Mmene Yobu anadziŵila Yehova . Yelekezani kuti mukuona Yakobo atate ake a Yosefe akumupukuta misozi mokoma mtima , kenako akumutonthoza pomulimbikitsa kukhala ndi ciyembekezo cimene cinatonthoza agogo ake a Abulahamu . Ndi nchito yosonkhanitsa iti imene ikuchulidwa pa Mateyu 24 : 31 ? ( b ) N’cifukwa ciani cocitika cakale cimeneci ndi nkhani yaikulu kwa ife ? Onani nchito imene imakhalapo kuti Baibulo lizipezeka m’zinenelo zambili . Safunanso kuti popemphela tizitsatila kakhalidwe ka thupi kapadela . Nanga bwanji ngati nchito imene munali kugwila inatha ndipo simukupezanso ina ? Baibulo imati : “ Cifukwa ca ucimo wa munthu mmodziyo [ Adamu ] imfa inalamulila monga mfumu ” kwa mbadwa za Adamu . Nkhani yotsatila idzafotokoza mmene tingacitile zimenezi . Komabe , kuuza ana anu kuti ici n’cabwino ici n’coipa , pakokha si kokwanila . Kodi Yesu anaphunzitsa ophunzila ake kuika maganizo ao pa ciani ? Nanga iye anapeleka citsanzo cotani ? ( a ) Kodi Malemba amaonetsa bwanji kuti kuphunzitsa ena n’kofunika ? Nanga nkhaniyi ikutikhudza bwanji tonsefe ? Mzimayiyo anati dzina lake ni Apun . Koma anali kucita zinthu mosamala cifukwa olo m’ma 1980 , nchito ya Mboni za Yehova inali yoletsedwa . Tikupemphanso abale onse amene angayenelele maudindo kuti akhale ofunitsitsa kuphunzila ndi kugwilitsa nchito zimene aphunzitsidwa pothandiza kusamalila nkhosa za Yehova . N’kutheka kuti m’maganizo mwake anati , ‘ N’cedwa pano , nifunika kucitapo kanthu mwamsanga . ’ Masiku ano , iye amalimbikitsa anthu kucita cidwi na ziŵanda poseŵenzetsa zipembedzo zonama na zosangalatsa zosiyana - siyana . Zinthu zabwino zimenezi ziphatikizapo zida , njila zolalikilila , ndi maphunzilo Tinali kuyewa banja lathu kwambili . N’taseluka sitima , n’nakwela basi yonipeleka ku South Lansing . Ndalama yolipilila n’nacita kukongola kwa winawake amene n’nakwela naye basi . Zotsatilapo zake n’zakuti Mabaibulo okonzedwanso a King James Version ndi Mabaibulo ena anacotsamo mawu olakwikawo . Nowa anali na ciyembekezo mwa Mulungu . ( Sal . 119 : 145 ; Maliro 3 : 41 ) Ngati zimativuta kufotokoza zimene zili mumtima mwathu , sitiyenela kutaya mtima , thandizo lilipo . Mu 1509 , Lefèvre anafalitsa buku loyelekezela buku la Masalimo kucokela m’mabaibo asanu a Cilatini . * Anafalitsanso Baibo ya Vulgate imene iye anakonza mbali zina zimene zinali zolakwika . Masiku ano , sindimenyanso anthu koma ndimawathandiza mwa kuwaphunzitsa za Mulungu . Kodi kusinkhasinkha Mau a Mulungu tsiku lililonse kumatipindulitsa bwanji ? Mwina mungaganize kuti anali wokamba - kamba ndi wopupuluma . Cifukwa cokonda anzao ndiponso mothandizidwa ndi mzimu woyela wa Mulungu , abale ndi alongo odzozedwa amenewo analalikila uthenga wabwino wa Ufumu mosasamala kanthu za mavuto amene anali kukumana nao . Yehova anatipatsa luso loti tizitha kuuza anzathu maganizo athu ndi mmene tikumvela . Kapena timafufuza mfundo za m’Baibo ndi kuyesetsa kuziseŵenzetsa , poonetsa kuti timadalila malangizo a Yehova pothetsa mavuto ? Citani zinthu modzipeleka osati mokakamizika . Lonjezo lakuti nkhondo siidzakhalakonso idzakwanilitsidwa mu Ufumu wa Mulungu . Taphunzila kuti Yehova amakamba ndi anthu mogwilizana ndi zocitika za panthawiyo . Palinso zinthu zina zabwino zimene munthu wina anan’citila zimene sinidzaiŵala . Timaonetsa kuti ndife omvela ndiponso okhulupilika kwa iye , ndipo kucita zimenezi kumathandiza kuti Mulungu ayankhe amene amamutonza . ( Miy . Laura , mlongo wosakwatiwa wocokela ku Canada , akutumikila monga mpainiya ku madzulo kwa dziko la Taiwan . Zaka zingapo zapitazo , mpainiya wina wa ku Germany , dzina lake Birgit , anapita kukapezeka pa mwambo wa otsiliza maphunzilo pamene mwana wake wamkazi anatsiliza maphunzilo . Machalichi ena ayesapo kulalikila mmene ife timacitila , koma alephela . ( b ) Tingasinkhesinkhe ciani tikamakonzekela utumiki ? N’zocititsa cidwi kuti m’kupita kwa nthawi , mwana woyamba wa Rakele , Yosefe , anakhala ndi ana aŵili aamuna Manase ndi Efuraimu . 34 : 10 ; 37 : 25 . Pamene ndinali ndi zaka 13 , ndinaganiza zophunzila Cijelemani . Lomba tidzakambilana mbali zitatu za mmene cikondi cathu cingayesedwele . Mbali zimenezi ndi ( 1 ) kukonda Yehova , ( 2 ) kukonda coonadi ca m’Baibo , ndi ( 3 ) kukonda abale athu . ( Rute 2 : 7 ) Rute anali na ufulu wokunkha , koma sanacite nawo dyela ufuluwo . Pa cifukwa cimeneci , io anataya zonse . Tiyeni tione njila zinayi . Pogwila Mau a Yehova kupitila mwa mneneli Yesaya , Yesu anati pokamba za iwo : “ Anthu awa amandilemekeza ndi milomo yokha , koma mtima wawo uli kutali ndi ine . “ PAMENE N’NALI MWANA , N’NALI KUMVA MAU OTUKWANA NA KUNYOZANA M’BANJA MWATHU . Nditangofika ku cipatala ca opaleshoni ca asilikali ku Mekong Delta , ku Dong Tam , kumene ndinafunika kuyamba kuseŵenza , ndeke za cipakapaka zambili zimene zinanyamula asilikali ovulala zinafika . Ngati timwetulila na kuwapatsa moni mwaubwenzi , angacite cidwi na khalidwe lathu komanso ndi Mulungu amene timalambila . Koma Yesu nthawi zonse anali kukamba mokoma mtima ndi mabwenzi ake . ( a ) Kodi aneneli anaonetsa bwanji kuti kudzabwela mtsogoleli wapadela ? N’cifukwa ciani tingakambe kuti Yehova wakhala akuthandiza amuna amenewo ? Nanga tidziŵa bwanji kuti akuthandiza kapolo wokhulupilika ndi wanzelu masiku ano ? Nanga tingaonetse bwanji kuti timayamikila kukhala na Mau a Mulungu m’citundu cimene timamvetsetsa ? Oyang’anila ndende anadziŵa kuti tinali okhulupilika . Panthawi yovuta imeneyo , n’nakumbukila mau a Yesu akuti : “ Ndinu odala pamene anthu akukunyozani ndi kukuzunzani . . . . Tikamudziŵa kwambili Yehova , sitidzakhumudwa ndi nkhani za m’Baibulo zimene sizifotokoza cifukwa cake iye anacita zinthu m’njila inayake . Atagwidwa cifundo , Yesu anayankha wakhateyo kuti : “ Ndikufuna . Kodi kungopeleka ndalama zothandiza panchitoyi kapena kuwalimbikitsa kugwila nchitoyi ndi kokwanila ? Cinanso , othandizawo afunika kupewa khalidwe limene lingapangitse anthu ena mumpingo kapena kunja kwa mpingo kuwakayikila . ( 1 Pet . Koma panthawi imodzi - modzi , tifunika kukumbukila kuti Yehova akhoza kuticitila zambili kuposa zimene tam’pempha , kapena zimene tinali kuyembekezela . * Kodi mfumuyo inacita ciani ? Onani nkhani ya mutu wakuti “ Kodi Mungadziŵe Bwanji Baibulo Lomasuliridwa Bwino ? M’bale Lemke , amene anali msilikali wa pamadzi , anapeleka lipoti lakuti anzake asanu anacita cidwi ndi uthenga wabwino . Akhristu oculuka adzimana zambili mu umoyo wawo kuti akhale na mpata wocita upainiya . wacinyengo ? KODI KUTSOGOLO KULI CIANI ? Yohane analembela kalata Gayo n’colinga cakuti amuyamikile . * Kodi simumasangalala ndi malonjezo amenewa ? Mulungu adzacotsapo zinthu zonse zobweletsa nkhawa . Sindife ochuka ndipo tilibe zinthu zambili zakuthupi , koma tili ndi Yehova , maphunzilo a Baibulo ndi zolinga za kuuzimu . Akhiristu odzozedwa amalimbikitsidwa na ciyembekezo cakuti adzalandila ‘ cisoti cacifumu cacilungamo . Ambuye , woweluza wolungama , adzapeleka mphotoyo m’tsikulo . ’ ( 2 Tim . Makolo anafunika kuphunzitsa ana awo pa mpata uliwonse umene apeza kuti naonso azitumikila Yehova yekha . — Deuteronomo 6 : 6 - 9 . Riana anakukadi , koma atangofika ku delalo anakumana na vuto . 115 : 3 - 8 ) Kodi maganizo akuti kulibe Mulungu amasoceletsa anthu zoona ? Komanso , anthu pofuna kupeza nchito yapamwamba , amacita zinthu mwampikisano , amakhala ansanje , ndipo pothela pake amangokhala ngati ‘ akuthamangitsa mphepo . ’ — Mlal . ( Yakobo 4 : 7 ) Conco , mukamagonjela Yehova mwa kumumvela na kumutumikila , mungakhale wotsimikiza kuti Satana na ziwanda zake sadzakuvutitsani . Kodi Yesu anatanthauza ciani pamene anakamba kuti tifunika kulambila “ motsogoleledwa ndi mzimu ndi coonadi ” ? 1 : 8 ) Kodi kuphunzila Baibo kungakuthandizeni bwanji kukulitsa khalidwe la kudziletsa ? Mungacite ciani kuti muzipindula kwambili poŵelenga Baibo ? Iye anati : “ Kuti tidziŵe ngati mau ali ouzilidwa ndiponso ocokela kwa Mulungu , timadziŵila izi : Mauwo amavomeleza zoti Yesu Kristu anabwela monga munthu . Palinso mtendele wina wamtengo wapatali . Pamene tinakhala atumiki a Mulungu , tinapanga masinthidwe aakulu amene anakhudza mbali zonse za umoyo wathu . Koma ife sitidziŵa . Cotelo , Cilamulo cinali ngati “ mtsogoleli ” wowafikitsa kwa Kristu . — Agalatiya 3 : 23 , 24 . Tikapitiliza kukhala okhulupilika kwa Yehova na gulu lake , tidzaona kukwanilitsika kwa mau okhudza mtima amenewa cifukwa tidzakhala na moyo mpaka muyaya . Anthu ambili akhala akutsutsana pa tanthauzo la mau opezeka m’Baibulo akuti , “ diso kulipila diso , dzino kulipila dzino . ” “ Mphatso iliyonse yabwino ndi yangwilo imacokela kumwamba , pakuti imatsika kucokela kwa Atate wa zounikila zonse zakuthambo , ndipo iye sasintha ngati kusuntha kwa mthunzi . ” — Yakobo 1 : 17 . N’takomboka kusukulu , anzanga angapo a m’kilasi ananimenya n’kunigwetsela pansi . Nkhani iyi ipeleka malangizo abwino ocokela m’Malemba , amene adzakuthandizani kukhala na zolinga zabwino zimene zingakuthandizeni kuti mtsogolo , mudzakhale na umoyo wabwino ndi wacimwemwe . Kukonzekeletsa Anthu ‘ Kuphunzila Zokhudza Yehova ’ N’nali nitangoyamba kumene giledi 2 . ( Kuyankha funso limeneli kutithandiza kukhala ndi cidziŵitso . ) Njila imodzi ndi mwa kukhala ndi zolinga za kuuzimu . Nkhani zimenezi zidzatithandiza kumvetsetsa lemba la 2 Timoteyo 2 : 19 , ndipo zionetsa kuti lembali limagwilizana ndi zocitika za m’nthawi ya Mose . Komabe , ofalitsa ambili nthawi imeneyo anafunika kuphunzitsidwa mmene angalalikilile . Zilizonse zimene munali kucita mu mpingo wanu wakale , n’zimenenso muyenela kucita mu mpingo watsopano kuti mukhalebe olimba kuuzimu . Ndithudi , kukamba mau olimbikitsa kungakhale na zotulukapo zabwino na zokhalitsa . ( Miy . Ndipo izi n’zoona . 2 : 9 ) Zoona , “ mphatso imene Mulungu amapeleka ndi moyo wosatha kudzela mwa Khristu Yesu Ambuye wathu . ” — Aroma 6 : 23b . Kenako , anayamba kuphunzila Baibo na Mboni za Yehova . Anthu amene anawagwila ukapolo anali kuwatonza . ( 1 Akor . 15 : 26 ) Onani mmene mayankho akuunikila cilungamo ca Yehova , nzelu zake , ndi cikondi cake makamaka . ( Aroma 10 : 4 ) M’maiko ena , okhulupilila anzathu amamwa zakumwa zoledzeletsa mosapitilila malile pa cakudya asanapite ku misonkhano . Sitinafune kutaya mwai umenewu ngakhale pang’ono . ” Pofotokoza Luka 13 : 24 , M’bale John Barr , amene anali wa m’Bungwe Lolamulila , zaka za kumbuyoku anati : “ Ambili amalephela kuloŵa pakhomo lopapatiza cifukwa sacita khama mokwanila . ” ( Onani ndime 16 - 19 ) Katswili wina wa matenda a maganizo anati : “ Njila yabwino yogonjetsela maganizo amenewa ndi kudziŵa kuti n’zacibadwa kumva conco , ndipo musamadziimbe mlandu mukakhala ndi maganizo amenewo . ” Tsopano imachedwa kuti Sukulu ya Alengezi a Ufumu . N’ciani cingakuthandizeni kupilila ngati wina m’banja mwanu wasiya Yehova ? Iye anamaliza ndi mau akuti : “ Pa zaka zonse zimene ndatumikila kuno , ndasangalala kwambili ndipo ndapeza mabwenzi ambilimbili . Nanga “ Gogi ndi Magogi ” wochulidwa pa Chivumbulutso 20 : 8 ndani ? Timafunanso kuceza ndi anzathu ndiponso kukhala ndi banja lacimwemwe . Pambuyo pa milungu ingapo , iye anayamba kubwela ndi bwenzi lake la cichaina kumisonkhano . N’ciani cimene mumaika patsogolo mu umoyo wanu ? Ndiye cifukwa cake tifunika kumasinkhasinkha pamene sindife otopa , tili pamalo acete , ndiponso pamene palibe zinthu zambili zosokoneza . M’malo mwake , tiyesetse kukhalabe okhulupilika mogwilizana ndi kudzipeleka kwathu pamene dongosolo la Satana lionongedwa . ( Yes . Iwo anali kupita ndi makalavani ao m’madela a mapili ndi m’zigwa , kuyambila ca kumpoto kwa Hokkaido mpaka kum’mwela kwa Kyushu . Muziwaphunzitsa makhalidwe abwino . Komabe , tingafunse kuti : Kodi cikumbumtima cabwino cingatithandize bwanji popanga zosankha ? Tidzakambilananso cifukwa cake cikondi n’cofunika kuti cikwati cikhale colimba . Conco ndinafuna kudziŵa zina zimene ndikanaphunzila . ” — Dennize , Mexico . Mungagwilitsile nchito nthawiyo kukulitsa mzimu wozindikila , wopatsa , wogwila nchito mwakhama , ubwino , kudzipeleka kwa Mulungu ndi kukhala ndi mbili yabwino . Lemba la Mlaliki 4 : 6 limati : “ Kupuma pang’ono kuli bwino kuposa kugwila nchito mwakhama ndi kuthamangitsa mphepo . ” Komabe , tinadziŵanso kuti io adzakumana ndi mavuto ambili popeza anali acinyamata . ” Nawonso anthu a Yehova masiku ano saika cizindikilo anthu amene adzapulumuka . Ambili mumpingowo anatumikila kwa nthawi yaitali , ndipo anali Akristu ofikapo kuuzimu . Mau awo anatilimbikitsa kuti tipite . ( Aroma 6 : 23 ) Kuti Mulungu amasule mtundu wa anthu ku cilango ca imfa , anatuma Mwana wake , Yesu Khristu , kubwela pa dziko kuti adzapeleke nsembe moyo wake wangwilo cifukwa ca anthu . Amuna ndi akazi mofunitsitsa anapeleka zopeleka zothandiza pa nchito ya Yehova . 23 “ Mau a Mulungu . . . Mulungu amafuna kugwilizanitsa zolengedwa zonse zimene ndi zomvela m’cilengedwe conse , ndipo adzakwanilitsa colinga cake cimeneci . Podzafika mu 1929 , cuma ca dziko lonse cinagwelatu . N’cifukwa ninji asayansi akangiwa kuyankha mafunso ambili ? Pa umoyo wathu wonse , ‘ nthawi zonse tizitsimikiza kuti covomelezeka kwa Ambuye n’citi . ’ ( Aef . Ndipo izi n’zimenedi amacita . — 2 Tim . Kodi Satana amacita ciani kuti atilepheletse kumva mau a Yehova ? ( Malaki 3 : 1 - 4 ) Kenako , m’caka ca 1919 , Yesu anasankha “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” kuti azipeleka “ cakudya pa nthawi yoyenela ” kwa anthu a Mulungu . Tinali kulalikila mwamantha cifukwa ukangomvela kuti injini ya ndeke yazima , udziŵa kuti posacedwapa ndeke idzaphulitsa bomba . Anthu amenewa anali kucokela m’dziko la Aisiraeli ndiponso m’dziko lililonse kumene kunali kukhala Ayuda . 1 : 15 - 17 ) Motelo , Yesu amacidziŵa bwino cilengedwe . Ndipo ndimapemphela kwa Yehova kuti adalitse khama lathu posamalila anthu oona mtima amene tawapeza kale . ” Pokambilana mavuto a m’banja , tisamaiŵale kupemphelela mzimu wa Yehova kuti utithandize kugwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo , ndi kuonetsa zipatso za mzimu wake . — Agal . 5 : 13 ) Ngakhale n’telo , iye angakumanebe ndi mavuto ena a m’banja . 5 : 9 , 10 ; 14 : 1 , 4 ) Mkazi amene akubeleka mbeu ndi “ Yerusalemu wam’mwamba , ” amene ndi mbali ya kumwamba ya gulu la Mulungu lopangidwa ndi zolengedwa zauzimu zokhulupilika . ( Agal . ( 2 Mbiri 11 : 13 , 14 ; 34 : 30 ) Conco mpomveka kukamba kuti ndodo ya “ Yuda ” inaimila mafuko aŵili a ufumu wakumwela . 37 ) , July ‘ MAU OSANGALATSA ATULUKA M’KAMWA MWA MFUMU ’ Kodi anthuwo akanacipeza bwanji cuma camtengo wapatali ca m’Baibo ? — Miy . N’zomvetsa cisoni kuti Aisiraeli anapandukila Mulungu wao , Yehova . Mlongo wina dzina lake Cynthia , * amene anasiidwa ndi mwamuna wake , anati : “ Cimapweteka kwambili ngati abale ako akukupewa kapena ngati sakucitila zinthu zimene umayembekezela anzako apamtima kukucitila . Ngakhale zili conco , Mulungu amaona anthu oona mtima amene amakonda zabwino ndi coonadi . Anthu adzayamba kutaya magalasi a maso , ndodo , njinga za olemala , ndi zipangizo zina za olemala . Conco ndinangodziuza kuti basi , kulibe Mulungu . Onani nkhani yakuti “ Munthu Amene Sadziŵa Zinthu Amakhulupilila Mau Alionse . ” Anthu amaona uthenga wathu m’njila zosiyanasiyana . N’cifukwa ciani kuyeletsedwa kwa Aroni ndi ana ake kuli ndi tanthauzo lalikulu kwa anthu a Yehova ? Kodi inasila nchito , kapena kodi ikali na malangizo othandiza kuposa mabuku ena onse ? Conco , pamene n’nanitanidwa ku Sukulu ya Giliyadi , n’nadabwa kwambili . ( Miy . 10 : 22 ) Olo kuti poyamba n’nali wosauka , lomba nalemela kwambili mwauzimu kuposa mmene n’nali kuyembekezela . Anakamba kuti kuciyambi kwa ulamulilo wake , zinthu padzikoli zidzaipila - ipila . Malemba amaonetsa kuti Yesu ndiponso Mulungu si olingana . N’cifukwa ciani kuvala cida ciliconse mwa zida zimenezi n’kofunika ? 11 : 23 - 27 ) Panthawi ina iye anazunzidwa ku Lusitara . 4 : 3 ) Mdyelekezi amatiyesa m’njila zambili koma tili ndi ufulu wosankha . Ngati sitinafotokoze zinthu momveka bwino , anthu sangamvetsetse kapena angakhulupilile zinthu zabodza . ( Luka 11 : 13 ) Ngati tipempha mzimu woyela ndi ‘ kupitiliza kuyenda mwa mzimuwo , ’ tidzayamba kucita zinthu mwacikondi kwambili ndi ena . M’banjali palibe woposa mnzake . Zimenezi sizitanthauza kuti kukhala osiyana ndi dziko kumakhala kopepuka nthawi zonse . ( b ) Fotokozani citsanzo coonetsa kuti ‘ mau a Mulugnu amathamanga kwambili . ’ Ataugonjetsa mzindawo , Koresi anamasula Ayuda amene anamangidwa ukapolo m’Babulo ndipo anawalola kubwelela kwawo kukamanganso Yerusalemu , amene anali ataonongedwa zaka 70 kumbuyoko Iye anati : “ M’kupita kwa nthawi , n’naona mapindu amene amabwela cifukwa cotsatila miyezo ya Yehova . Izi zikuonetsa kuti mumakonda kwambili Mau a Mulungu . Pa nthawi imeneyo aliyense mwa anthu a mtundu wako amene dzina lake lidzakhala litalembedwa m’buku adzapulumuka . ” ( Dan . ( 1 Samueli 25 : 2 ; 2 Mafumu 3 : 4 ; Yobu 31 : 20 ) Mbeu za fulakesi zopangila nsalu zinali kulimidwa ku Iguputo ndi ku Isiraeli . Popeza iye ni Gwelo la moyo , amakhala Tate wa aliyense woukitsidwa . ( Sal . MBILI YANGA : WONYADA , WAMTIMA WOSAFUNA KUUZIDWA ZOCITA Zekariya anafunsa kuti , “ Kodi magaleta amenewa akuimila ciani ? ” ( a ) Ulosi wa Yesaya wokhudza Yerusalemu unakwanilitsidwa liti ? 6 : 1 - 3 ; Chiv . Mwacitsanzo , m’bale wina ku Thailand anati : “ Nchito yanga yokonza makompyuta n’nali kuikonda ngako , koma n’nali kufunika kuseŵenza maola ambili . Pa msonkhano wa pacaka wa mu 2016 wa Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania , abale na alongo anasangalala ngako pamene M’bale Stephen Lett wa m’Bungwe lolamulila , analengeza kuti pamisonkhano tidzayamba kuseŵenzetsa buku la nyimbo latsopano lakuti , ‘ Imbani Mokweza ndi Mosangalala ’ kwa Yehova . Sascha , m’bale wokwatila wa zaka za m’ma 40 wocokela ku Germany , anati : “ Nthawi zonse nikapita mu ulaliki , nimakumana ndi anthu amene n’koyamba kumvelako coonadi . N’zokondweletsa kuona acinyamata akutenga maudindo aakulu ( Onani palagilafu 9 ) Dustin amene akutumikila pa Beteli anati : “ N’nakhala na colinga cocita utumiki wanthawi zonse nili na zaka 9 , ndipo n’nayamba upainiya n’tatsiliza sukulu . Kutengela maganizo aconco , m’kupita kwa nthawi kungafooketse cikhulupililo cathu . Iwo amakamba kuti , ‘ munthu aliyense amabadwa na kufa , ndiye mmene moyo ulili . ’ Mwacitsanzo , usiku wakuti maŵa aphedwa , ophunzila ake anali kukangana pakati pao “ za amene anali kuoneka wamkulu kwambili . ” ( Yesaya 40 : 29 ) Mtumwi Paulo amene anapilila mayeselo aakulu anakamba kuti : “ Pa zinthu zonse , ndimapeza mphamvu kucokela kwa iye amene amandipatsa mphamvu . ” Yesu sanakumbutse ophunzila ake zolakwa zawo , ngakhale zimene iwo anacita pamene iye anamangidwa . Yesu anaonetsa kuti atumiki a Mulungu angapemphele ndi mtima wonse kuti : “ Mutipatse ife lelo cakudya cathu calelo . ” Mai wina dzina lake Katia amene alela yekha mwana anati , “ Kale ndinali wosadekha ndi mwana wanga wamkazi . Nalonso lemba la Aroma 15 : 5 limanena kuti tifunika kukhala na “ maganizo amene Khristu Yesu anali nawo . ” Nthawi zina , abale ocokela ku mipingo ina anali kubwela kudzapeleka nkhani ya onse , ndipo tinali kufunafuna malo alendi . Tiyenela kugwilitsila nchito mafanizo osavuta kumva . 2 : 1 , 2 , 4 - 12 ) Lilime lathu limakhala monga “ colembela ca wokopela malemba waluso ” cifukwa cakuti timagwilitsila nchito kwambili Mau olembedwa pa nchito yathu yolalikila . Ngakhale kuti Yesu nayenso anali wolema , anakhala maso mwa kulimbikila kupemphela kwa Atate wake . 16 : 32 ) Komabe Yehova anali kulamulilabe monga mmene anali kucitila m’nthawi yakale . Tsopano , iye wakhala bwenzi langa lapamtima . Liu la cinenelo coyambilila ca Baibo limene linamasulidwa kuti “ zinthu zodetsa ” limaphatikizapo zinthu zambili , osati cabe macimo okhudzana ndi zaciwelewele . Mwina iye angagonjele n’kucita zimene imwe mufuna , koma kodi kucita zimenezi kungam’thandize kukopeka naco coonadi ? Pa May 11 , mu 1985 , ndinamasulidwa ku ndende ya Dzaleka . 69 : 28 . Kodi ciyembekezo cili monga cisote ca msilikali m’lingalilo lanji ? Mneneli Yesaya ndi Yeremiya analoselapo za mgwilizano umenewu . — Yes . Conco , n’nali kucita kumasulila nkhani za m’Cirasha kuti abale amvetse coonadi mosavuta . Anthu m’maikowa ali ndi zikhalidwe ndi miyambo yosiyanasiyana . Kukamba zoona , palibe munthu ayenela kutamandidwa cifukwa comvetsetsa ndi kufotokoza bwino “ zinthu zozama za Mulungu . ” Coyamba , bwanamkubwa waciroma Florus akulanda ndalama zokwana matalente 17 zocokela m’thumba la kacisi wopatulika . Iye anali kufuna kuwaphunzitsa mfundo inayake yofunika kwambili . Iye anapempha Atate wake wakumwamba kuti athandize otsatila ake kukhala ogwilizana monga mmene iye alili wogwilizana ndi atate wake . — Yohane 17 : 21 , 22 . Onse akugwila nchito yolalikila mogwilizana . Mosiyana na zimenezi , anthu amene amakonda Mulungu , amakhala na makhalidwe abwino . Pambuyo pake , mu 1994 , Mboni ku Rwanda zinakana kuloŵelela m’nkhondo yofuna kuseselatu mtundu . Mpainiya wina dzina lake Bobbi , anacondelela kuti : “ Mkati mwa mlungu timafuna anthu ambili olalikila nao . ” Aliyense wa io wakhala mu utumiki wanthawi zonse kwa zaka zoposa 20 . “ UMUNTHU WATSOPANO . ” M’malo mosunga cakukhosi , tsatilani citsanzo ca Petulo . — Mlal . Tikuitanilani inuyo , a m’banja lanu , ndiponso anzanu , kuti mudzapezekepo ndi kumvetsela nkhani ya m’Baibulo . Lembali likusonyeza kuti ubwenzi wathu ndi Mulungu umadalila pa mbali ziŵili . N’ciani cingacititse kusamvana pakati pa ise na acibululu amene si Mboni ? Zolinga zingakwanilitsidwe m’nthawi yocepa ( zotenga masiku kapena ma wiki kuti zikwanilitsidwe ) , kapena m’nthawi yotalikilapo pang’ono ( miyezi ) , komanso zotenga nthawi yaitali ( caka kapena kupitililapo ) . Kodi anthu ena anakamba ciani ataona Nyumba za Ufumu ndi anthu amene anasonkhana pa nyumbazo ? M’zaka zokafikitsa ku nkhondo yoyamba ya dziko lonse , Charles Taze Russell na anzake anazindikila kuti Machechi Acikhiristu sanali kuphunzitsa coonadi ca m’Baibo . Pamene gulu la ngamila linali kudutsa m’dziko la Negebu , dzuŵa likuloŵa , Rabeka anaona mwamuna akuyenda m’chile . NYIMBO : 150 , 10 Olo kuti n’nakulila m’banja laconco , sin’nakhale wa cipani ca Nazi kapena sisitele . ( Ŵelengani Chivumbulutso 6 : 1 , 2 ) Ulosi umenewu unanenelatu kuti pambuyo pakuti Ufumu wa Mulungu wayamba kulamulila , zinthu padziko lapansi zidzaipilatu . Zaka za m’ma 400 , katswili wina wacigiliki dzina lake Plato , m’buku lake lina anati : “ N’zovuta kwambili kudziŵa amene anapanga ndiponso tate wa cilengedwe cathu . Ngakhale titam’dziŵa , zingakhale zosatheka kuuzako aliyense za iye . ” Taphunzila kudalila Mulungu panthawi zovuta , ndipo taona kuti nthawi zonse Iye wakhala akuthandiza ndi kulimbitsa banja lathu . — Salimo 55 : 22 . Mwacitsanzo , mukamakonzekela kukacititsa phunzilo la Baibulo , muzipeza nthawi yosinkhasinkha . Takamba conco cifukwa cakuti mtumwi Paulo anawachula kuti “ abale 500 . ” Koma mwadzidzidzi , Eliya anamufikila . Atsogoleli aciyuda ndiwo “ omanga nyumba ” amene anakana Mesiya . Iwo anam’kana Yesu kuti si Khristu . N’nakondwela ngako cifukwa n’nayamba kumvetsetsa coonadi ca m’Baibo . Ndipo Manda a anthu onse akutsatila pafupi , kutenga miyoyo ya anthu ambili . — Chivumbulutso 6 : 1 - 8 . N’cifukwa cake ingakhale ngozi yaikulu kwambili ngati tingagonje ku zikhumbo zoipa monga mmene zinakhalila ndi Aisiraeli 24,000 m’cigwa ca Moabu . Pa msonkhano wa cigawo wa mu 2005 , Thierry na mkazi wake Nadia anaonelela seŵelo la mutu wakuti , “ Yesetsani Kukwanilitsa Zolinga Zimene Zimalemekeza Mulungu . ” Mbili Yanga Jairo Amagwilitsila Nchito Maso Ake Potumikila Mulungu 13 Paulo anati : “ Pali mgwilizano wotani pakati pa Kristu ndi Beliyali ? NJILA YOTHETSELA VUTOLI : Bungwe lina lolimbana ndi ziphuphu linanena kuti maboma afunika kuphunzitsa anthu kukhala “ okhulupilika , oona mtima , ndi odalilika ” kuti akwanitse kuthetsa ziphuphu . Nkhope ya ubwenzi ya Yesu na khalidwe lake labwino , zinacititsa ciitano cake kukhala cokopa makamaka kwa anthu “ ogwila nchito yolemetsa ndi olemedwa . ” N’tasoŵa cocita , n’namvela zimene iye ananiuza ndipo n’naleka kuphunzila na Mboni . Umboni wina waukulu ndi wakuti Yesu ataukitsidwa anawonekela kwa anthu ambili pa malo osiyanasiyana ndiponso pa nthawi zosiyanasiyana . Zinthu zikamasintha paumoyo wathu , timafunika kukhala ndi makhalidwe amenewa . YEHOVA anaonetsa mphamvu zake kudzela mwa Yesu Kristu ndipo anacita zimenezi m’njila zapadela kwambili . Koposa zonse , anali kudziŵa mavuto amene ophunzila ake anali kukumana nawo panthawiyo . 31 : 1 - 6 . ) Conco , timakonda Mulungu “ cifukwa iye ndi amene anayamba kutikonda . ” — 1 Yohane 4 : 19 . Muuzeni colinga cimene munali naco , ndipo mufotokozeleni mogwila mtima cisangalalo cimene munapeza mutakwanilitsa colingaco . Pambuyo popenyelela “ Seŵelo , ” anthuwo anawapatsa tumabuku twa Seŵelo la Cilengedwe . Komanso , kodi mungawathandize bwanji alendo amene akukila mu mpingo wanu kuti zisawavute kujaila ? Koma kodi muganiza kuti “ Wam’mwambamwamba ” ameneyo ndani ? Sikuti ni Yesu cabe amene anadzudzula Ayuda cifukwa ca khalidwe limeneli . Kumeneko , n’nali kulalikila m’citundu ca Cihangare . ” Potifara anali kumudalila kwambili Yosefe , koma Yosefe tsopano ali m’ndende cifukwa cakuti mkazi wa Potifara anamunamizila kuti anafuna kumugwililila . ( a ) Tingacite ciani kuti Satana asatifooketse ? ( 2 Tim . 3 : 1 - 5 ) Cikondi cathu pa Yehova ndi kufunitsitsa kwathu kutsatila miyezo yake , zimayesedwa tsiku lililonse . N’zoona kuti kukhala wodziletsa pa zocitika ngati zimenezi si kopepuka . ( Mlaliki 7 : 12 ) Kukhala na cidziŵitso komanso nzelu zocokela kwa Mulungu , kungatiteteze m’nthawi ino na kutithandiza kupanga cosankha canzelu cimene cingatitsogolele kukapeza moyo wosatha m’tsogolo . Mofananamo , mwina tatumikila Mulungu m’gulu lake kwa zaka zambili . Ngati mukambilana ndi wacinyamata , mungayambe makambilano anu mwa njila iyi : “ Ndifuna kukuŵelengela lemba limene lili ndi funso lofunika kwambili . Nthawi yoyamba pamene Yesu anali kuuza ophunzila ake kuti azikumbukila imfa yake , anachula za pangano . Kumbukilani kuti Yesu anauza ophunzila ake kupemphela kuti : “ Ufumu wanu ubwele . Rocio anafotokoza kuti : “ Patapita mwezi umodzi pambuyo posamukila m’kanyumba kakang’ono , tinaitanidwa kukatumikila ku Wallkill monga ogwila nchito pa Beteli amene amayendela . Ngati zili conco , ndiye kuti pali cifukwa cimene anatipangila . Yesu anati : “ Inu munamva kuti anati , ‘ Uzikonda mnzako ndi kudana ndi mdani wako . ’ Mukacita zimenezo , mudzaonetsa kuti ndinu wokhulupilika kwa Yehova . Zimakhala zovuta kwa atumiki a Yehova ena kupeza ndalama zokwanila zogulila zinthu zofunika pa umoyo . ( b ) N’cifukwa ciani sitiyenela kuimba mlandu ena tikakumana ndi mayeselo ? Tsiku limenelo tinaphunzila mitu itatu m’buku la Coonadi , ndipo tinayamba kukondana kwambili ndi m’bale Gardner . Kodi alongo acikulile angaonetse bwanji kulimba mtima ? Yesu anati : “ Aliyense wocita chimo ndi kapolo wa chimo . . . . Mulimonse mmene zingakhalile , ululu wa imfa sitingaupewe , ndipo zotsatilapo zake zimakhala zophweteka kwambili . Baibulo limanena kuti , “ M’tsogolo , anthu oipa adzaphedwa . ” — Salimo 37 : 10 , 38 ; Danieli 2 : 44 . Anamuuza kuti adzawonjezela katatu malipilo amene anali kulandila . N’cimodzi - modzi na zosangalatsa . Kucita zosangalatsa zabwino pa mlingo woyenela kulibenso vuto . Iye anafuna kuphunzila zoonjezeleka kwa Mphunzitsi Wamkulu . Khalani wopatsa 1 : 14 ) Satana amaseŵenzetsa zipembedzo zabodza kuti acititse khungu maganizo a anthu . Komabe , adzaphunzitsa anthu omvela njila zake , ndi kuwathandiza kusintha maganizo ao ndi zocita zao zoipa . Kodi Mkhristu amene walapa safunika kukayikila za ciani ? 65 : 2 ) Kuwonjezela apo , tikazindikila kuti Yehova amayankha mapemphelo athu , cikondi cathu pa iye cimakula . N’ciani cinathandiza Yosefe kuti asagonje ? 61 : 1 ) Mlongo Charlotte , amene watumikila mu utumiki wanthawi zonse kwa zaka 38 , anati : “ Anthu masiku ano ni osocela . Mtumwi Paulo anati : “ Khalani ndi maganizo amenewa , amenenso Kristu Yesu anali nao . ” ( Afil . Iye anati : “ Tsopano ndimapeza ndalama zocepa kuyelekezela ndi zimene ndinali kupeza nditapita ku dziko lina . ( a ) Kodi tingalimbitse mgwilizano wathu m’njila zitatu ziti ? N’ciani cathandiza Jason kupilila ? Kapena muona kuti ndinu okonzeka , koma makolo anu akuuzani kuti muyembekeze coyamba kuti mukuleko ndi kudziŵa zambili . Abulahamu anali ndi cikhulupililo cakuti panthawi ina iliyonse , Yehova akhoza kuukitsa Isaki kuti malonjezo ake onse akwanilitsidwe Tiyeni tikambilane zinthu 9 zimene tingacite zoonetsa kuti tili na cikondi “ copanda cinyengo . ” Ngakhale kuti mfumu inali kumukopa , iye sanafune kusintha maganizo ake . Msulami anali kufuna kukwatiwa ndi m’busayo basi . ( c ) N’ciani cimene tingacite kuti tipite patsogolo mwauzimu ? Anthu ambili m’machechi amaphunzitsidwa kuti kwawo kweni - kweni kokakhala ni kumwamba , osati m’paradaiso padziko lapansi . Kodi pali winawake amene akundimvetsela ? ’ Mmodzi wa acicepelewo tsopano akutumikila m’Komiti ya Nthambi , ndipo ena aŵili ni apainiya apadela . Onani zitsanzo zina za anthu amenewa monga Lillian Gobitas Klose , mu Galamukani ! Mu July 1943 , inenso n’nakhudzidwa . Ŵelengani Malaki 3 : 16 . Patapita zaka zoposa 30 pangano la Abulahamu litayamba kugwila nchito , pang’onopang’ono Yehova anaulula mbali yofunika ponena za mbeu ya mkazi . N’cifukwa Ciani Pali Osiyana - siyana ? Kodi acicepele , makolo , alongo acikulile , ndi abale obatizika angaonetse bwanji kuti ni olimba mtima ndi kuti ni okonzeka kugwila nchito zabwino ? Tiyelekezele conco : Ganizilani tate amene akuphunzitsa mwana wake kuyendetsa motoka . Cimwemwe cimatanthauza , “ kumva bwino mu mtima cifukwa copeza kapena kuyembekezela zabwino . ” 5 : 7 . Zimene Ufumu Wa Mulungu Udzacita ? Timoteyo anagwila nchito ndi mtumwi Paulo , bwenzi lake , kwa zaka zoposa 14 . 8 : 14 , 15 ) M’kupita kwa nthawi , akulu ena odzozedwa anayamba kuthandiza atumwi kutsogolela mipingo . Tsiku lina , dokota wina wacikulile amene anali wa Mboni za Yehova , dzina lake Fred Hardaker , anabwela ku nyumba kwathu . Cacitatu , aliyense wa ise amaloŵetsedwamo m’nkhani ya kukhala wokhulupilika . Iye anali kudziŵa bwino mfundo za m’Cilamulo ca Mose , ndipo mfundozo zinakhudza mmene anali kucitila zinthu ndi anthu . Pang’ono - pangono n’naphunzila kucita zimenezi . Woyang’anila ndende anacita mantha poganiza kuti akaidi athaŵa . Akuti katswili panchitoyo zinali kum’tengela miyezi 10 kukopa Baibo imodzi cabe . Kodi kucitila cifundo ndi kukomela mtima onse mumpingo kungakhale na zotulukapo zabwino ziti ? Tingathandize panchito yokulitsa paladaiso wauzimu ( Onani ndime 18 ndi 19 ) Antonio wa zaka 32 anati : “ Ndikamva Jairo akupeleka ndemanga pamisonkhano , ndimalimbikitsidwa . ” 2 : 19 , 20 ; Luka 21 : 20 - 22 ) Tsiku la Yehova limenelo linafika mu 70 C.E . pamene Aroma anawononga Yerusalemu mogwilizana na ciweluzo ca Yehova . Komanso , madzi tinali kutapa pacitsime . Popeza kuti ndi wokwiya kwambili , iye akucita zilizonse zimene angathe kuti aticititse kukhala wosakhulupilika . Abale ndi alongo amenewa angakhale ndi maganizo ofooketsa cifukwa ca matenda , ukalamba kapena zokhumudwitsa . ( Sal . 71 : 9 ; Miy . 13 : 12 ; Mlal . ( Luka 22 : 41 , 43 ) Mwamuna wina wokhulupilika Nehemiya , anaopsezedwa ndi anthu oipa amene anayesetsa kumuletsa kugwila nchito ya Mulungu . Mkristu woganiza bwino sakakamiza ena kucita zimene iye akuona kuti n’zabwino . Ambili amafunsila kwa anthu amizimu kuti adziŵe zakutsogolo . N’cifukwa cake timapitiliza “ mwakhama kuphunzitsa ndi kulengeza uthenga wabwino wonena za Kristu Yesu , ” mmene anacitila Akristu oyambilila . — Machitidwe 5 : 41 , 42 . Ndi mbali iti ya cizindikilo imene ikusonyeza kuti tikukhala m’nthawi ya mapeto ? N’nabadwa pa November 9 , 1929 mu mzinda wa Sukkur , m’dziko limene lomba limachedwa Pakistan . Mzindawu uli kumadzulo kwa mtsinje wa Indus . M’caputala 6 ca Aefeso , ndinaphunzila kuti Yehova amafuna kuti ndizimvela makolo anga . ( 1 Sam . 13 : 13 , 14 ) Panthawi yake , Mulungu anasankha wina wake amene anali kudzakhala wapamwamba kupambana amuna amene anagwilitsidwapo nchito . Komabe , Paulo anaona nsembeyo ngati mphatso yake yopatsidwa ndi Mulungu . Kodi tiphunzilapo ciani pankhaniyi ? Anali kudalila “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , amenenso amatitonthoza m’masautso athu onse . ” ( 2 Akor . Anthu mamiliyoni ambili amene anamwalila , adzakhalanso ndi moyo . Titalalikila kwa miyezi ingapo ku zisumbu za ku Bahamas , tinasamukila ku zisumbu za Leeward ndi Windward zimene zili pam’tunda wa makilomita 800 kucokela ku zisumbu za Virgin . Zisumbu zimenezi zili pafupi ndi Puerto Rico ndipo zimayandikila ku Trinidad . Nanga bwanji pamene munaceleza abale na alongo ena a mu mpingo mwanu , kodi ubwenzi wanu na iwo sunalimbe ? Abale na alongo anayeletsa sitediyamu imeneyi , wiki yonse msonkhano usanafike . N’nayambanso kuphunzila Baibulo ngakhale kuti panali patapita zaka 20 . Ngati n’conco , pezani nthawi yosinkhasinkha cifukwa cake mumakhulupilila zimene munaphunzila . Baibulo limafotokoza makonzedwe a kucotsa munthu mumpingo kumene kumakhala ndi zotsatilapo zosangalatsa . A SERGIO na akazi awo a Olinda ni apainiya a zaka za m’ma 80 , ndipo amakhala ku America . N’zoona kuti , kuti ukapolo wa mtundu uliwonse uthe , padzafunikila masinthidwe aakulu pakati pa anthu . Ciwombankhanga Komabe , tisaiŵale kuti pali zinthu zina zofunika kwambili zokhudza Paulo kuposa maonekedwe ake . Inanenanso kuti , “ mtsogolomu zioneka kuti padziko lonse , mmodzi pa akazi 5 adzakakamizidwa kugonedwa . ” Ndimakonda kuŵelenga lemba la Afilipi 4 : 6 , 7 . Pamene anali kuphunzila , Tessie anafotokozela mlongo amene anali kumuphunzitsa cifukwa cake sanali kupita patsogolo kuuzimu . Kuwonjezela apo , imaika paudindo oyang’anila dela , amene nawonso amaika akulu . Lonjezo la Yehova lakuti adzatulutsa mbeu imene idzadalitsa mitundu yonse ya anthu inali kudzakwanilitsika kupitila mwa mwana wa Sara . Webusaiti yathu ya jw.org na zofalitsa zina , zili na nkhani zimene zinakonzedwa kuti zithandize acicepele kudziŵa mmene angayankhile mafunso ofunsidwa kaŵili - kaŵili , monga yakuti , “ N’cifukwa Ciani Mumakhulupilila Kuti Kuli Mulungu ? ” Kuyambila mu 2011 , amene amaitanidwa ku sukuluyi ndi apainiya apadela , oyang’anila oyendela , atumiki a pa Beteli , ndi amishonale amene sanaloŵepo sukuluyi . Conco , kupanga zosankha mwanzelu kungatithandize kukhala na umoyo wabwino ndi wamtendele , m’malo mokhala na umoyo wosasangalala , wodzala na mavuto . — Miy . Kodi ufulu weni - weni unatayika bwanji ? SAULI ndi asilikali ake 3,000 , anali kufunafuna Davide m’cipululu ca Yuda kuti amuphe . N’cifukwa ciani sitiyenela kuleka kulimbikitsa ena ? 102 : 7 ) Mukakhala ndi maganizo amenewo , tulilani Yehova nkhawa zanu monga anacitila wamasalimo . Mapemphelo anu angakuthandizeni polimbana ndi maganizo olakwika . ( Salimo 83 : 18 ) Mbonizo zinandionetsa lemba la 1 Timoteyo 4 : 8 , limene limati : “ Kucita maseŵela olimbitsa thupi ndi kopindulitsa pang’ono , koma kukhala wodzipeleka kwa Mulungu n’kopindulitsa m’zonse , cifukwa kumakhudza lonjezo la moyo uno ndi moyo umene ukubwelawo . ” Kudziŵa dzina la Mulungu ndi cinthu coyamba cimene mungacite kuti mukhale naye paubwenzi . — Yakobo 4 : 8 . M’dziko lina limene nchito yathu ni yoletsedwa , abale amapeleka nyumba zawo kuti zizigwilitsidwa nchito monga Nyumba za Ufumu . Izi zathandiza kuti apainiya ndi abale ena amene ali na ndalama zocepa akhale na malo olambilila aulele m’malo mocita lendi . Inde , ndipo m’Baibulo muli nkhani zambili zoonetsa kuti Mulungu amathandizadi . N’cifukwa ciani amene atumikila mumpingo wa cinenelo cina amapindula ngati aphunzila Baibo m’cinenelo ca kwawo ? Mosakaikila , io anacita cidwi kuona mmene mnyamatayu anali kupitila patsogolo , ndiponso mmene analili citsanzo cabwino kwa ena . Nanga bwanji inu acinyamata amene mufunika kuthandiza mpingo ? Zoonadi , coonadi ca m’Baibulo cinandithandiza kupeza mayankho okhutilitsa . Pamene anali m’cipatala , anali kulalikila madokota , odwala , ndi alendo okaona odwala . Koma ganizilani izi : Masiku ano , aliko munthu wamtali mamita 2.7 . Iye walonjeza kuti : “ Olungama adzalandila dziko lapansi , ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya . ” Zimenezi zicitike kuti moyo wosatha ubwele kudzela mwa Yesu Khristu Ambuye wathu . ” — Aroma 5 : 20 , 21 . Cifukwa colephela kudziletsa , iye analankhula mosasamala popanda kuganizila zotulukapo zake . Iye anafuna kuti io azidalila Yehova amene amapeleka madalitso osatha . 21 : 1 , 2 . Ngati mwamuna amacita umutu wake mwacikondi monga Yesu , sicikhala covuta kwa mkazi wake kum’konda , kum’lemekeza , ndiponso kulemekeza zosankha zake . — Ŵelengani Tito 2 : 3 - 5 . Pamene m’badwo wina ucoka ndipo wina ubwela , acinyamata amatenga nchito za acikulile . Ndinavomela ndipo tinapangana kuti pa Cinai m’maŵa tikayambe kuphunzila Baibulo . Ndi mfundo zofunika kwambili ziti zimene tiyenela kukumbukila tikakhala pa misonkhano ? Zimenezi n’zofunika ngati tinalandiladi cisomo ca Mulungu , ndiponso ngati ‘ ucimo suli mbuye kwa ife . ’ Zimenezi zinali kucitika tsiku lililonse kwa miyezi iŵili . ( Luka 4 : 13 ) Yesu sanagonje pa mayeselo onse a Satana ofuna kuononga kukhulupilika kwake . ( 2 Timoteyo 3 : 1 - 5 ) Kodi mudzayesetsa kudziŵa tanthauzo la ‘ nthawi ’ ino mofanana ndi dokowe amene amadziŵa nthawi yake yokuka ? Mwacionekele , iwo adzakufotokozelani zocitika zolimbikitsa . — Aef . Kwa nthawi yoyamba pa umoyo wanga , ndinayamba kudziletsa pa zocita zanga . Ukwati wathu wakhala wolimba kwambili cifukwa tonse aŵili timagwilitsila nchito malangizo a m’Baibulo . Wokwelapo akuimila njala . Onetsetsani kuti zocita zanu ( nchito , sukulu , zosangalatsa , na zina ) zimakupatsani mpata wokwanilitsa zolinga zanu zauzimu . — Aef . ( Mateyu 20 : 2 ) Ndalama imodzi - modziyo ingagule makilogalamu atatu a balele , cakudya cimene anthu sanali kucikonda poyelekeza ndi tiligu . 25 : 16 . Conco , m’malo mowauza kuti adzakhala mboni za Yehova , iye anawauza kuti adzakhala mboni zake . Ophunzila a Khristu oyambilila amenewa , ayenela kuti anasonkhezeledwa na nzelu za dzikoli . Ndi mfundo ziti za m’Baibulo zimene zingakuthandizeni kusangalala ndi nchito yanu ? ( Nehemiya 9 : 17 ; Salimo 86 : 5 ) Ngati timayamikila cifundo ca Yehova , nafenso tidzacitila cifundo anthu ena mwa kuwakhululukila mocokela pansi pamtima . 38 : 10 - 12 ; Mika 5 : 5 , 6 ) Cifukwa ca ici tikupempha akulu nonse kuti muyambe lelo kuphunzitsa ena ndi kuona nchitoyi kukhala mbali yofunika ya utumiki wanu . Kuona moyo kukhala wamtengo wapatali ( Yesaya 2 : 4 ) Popeza kuti Yehova walola kuti maboma a anthu azitilamulila , sitilimbana nao kapena kuwatsutsa . Wolemba mbili wina ananena kuti asilikaliwo “ anazunzika ndi kuvutika maganizo kwambili pankhondoyo kuposa ndi kale lonse . ” Iwo ni ena mwa “ anthu amene , mwa cikhulupililo ndi kuleza mtima , akulandila zinthu zimene Mulungu analonjeza monga coloŵa cawo . ” Kapena tingafune kupeza “ zinthu zazikulu ” mwa kucita maphunzilo apamwamba . Monga mmene Yehova anathandizila Solomo , nafenso akhoza kutithandiza kukhala olimba mtima ndi kugwila nchito yathu m’banja ndi mumpingo . ( Yes . Akulu mumpingo amagwilitsila nchito nthawi yao pocita zinthu mwakhama kuti ife tipindule . Ulosi umenewo unalembewa kukali zaka zoposa 1,000 , ndipo unakwanilitsika . Pali pano , ku India kuli Mboni za Yehova zacangu zoposa 37,000 , ndipo anthu oposa 108,000 anapezeka pa Cikumbutso caka catha . Kucita izi kumapangitsa kuti ena aziwalemekeza ndipo kumawapatsa ufulu wa kulankhula pophunzitsa na kulangiza ena . Abale ambili sanali kudziŵa kulankhula pa gulu la anthu . Komabe , cinthu cina cinayamba kutenga malo paumoyo wanga . TSAMBA 19 • NYIMBO : 98 , 104 Koma tsopano tiyeni tikambilane njila zinai zimene zingatithandize kukonda kwambili Yehova , komanso mmene tingaonetsele kuti timam’konda . 3 : 1 ) N’kuthekanso kuti talema ndi kuona makhalidwe oipa a anthu amene timakhala nawo pafupi . Tikatelo , anthu adzalemekeza Mulungu cifukwa ca makhalidwe athu abwino m’malo molemekeza ise . ( Genesis 24 : 39 , 41 ) Banja la Betuele linali kulemekeza ufulu wa mtsikana . Paulo anaonetsa kuti cikondi n’cofunika kwambili pakati pa Akristu . Iye anati : “ Valani cifundo cacikulu , kukoma mtima , kudzicepetsa , kufatsa , ndi kuleza mtima . ( Sal . 37 : 25 ) Komabe , panthawi yovuta imeneyo iye anadziŵa kuti Yehova sanamusiye . Ndife osangalala kwambili kuti tikukhala m’nthawi imene ‘ anthu ozindikila awala ’ kwambili . Nkhondo ya Aramagedo idzathetsa nkhondo zonse . — Salimo 46 : 8 , 9 . Ena anali ndi khalidwe laciwelewele . Gulu lina la oimba nyimbo linatulutsa cimbale ca nyimbo zochuka cimene anacipatsa dzina lakuti Wokana Kristu . Posakhalitsa , anazindikila kuti panalibe cipembedzo olo cimodzi cimene cinali kutsatila Mau onse a Mulungu . Kodi Mulungu ndi wotani ? Kodi Yehova anathandiza Yobu kuzindikila ciani ? Nanga Yobu anacitapo ciani ? ( Yoh . 18 : 36 ) Popeza kuti pa kampaniyi tinali kukonza sitima za pamadzi zankhondo , n’nasankha zosiya nchitoyi ndi kuyamba utumiki wa nthawi zonse . ( a ) Ni vuto lanji limene Rakele anali nalo ? Koma ngati wina mumpingo wacita colakwa cacikulu , ndi bwino kupempha thandizo kwa akulu ndi kuwadziŵitsa za colakwaco . Iye anati : “ Ndinaleka kukoka cifukwa cophunzila Baibulo . Conco , zinali zovuta kuti apange cosankha . Komabe , Baibo imafotokoza mosapita m’mbali kuti “ nsanje yaikulu ndi kukonda mikangano , ” zingawononge ubwenzi wathu na ena ndi kuyambitsa mavuto mumpingo . ( Yak . Conco , m’bale mmodzi anaikidwa kuti akhale kalinde . Koma makonzedwe amenewa atiphunzitsanso za makhalidwe a Yehova , na zimene tingacite kuti titengele citsanzo cake . Olaf anati : “ Nditakoka ndudu nthawi yoyamba , ndinaona ngati kuti panalibe vuto lililonse . Kodi “ mau a Mulungu ” n’ciani ? Njila imodzi imene angelo amatumikila Mulungu ndi kuthandiza pa nchito yofunika kwambili imene ikucitika padziko lapansi masiku ano , yolengeza uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . Zocitika monga zimenezi zapangitsa kuti nizikhala wokondwela kwambili na utumiki wanga kuno . ” DZIKO : CANADA Ndipo ndidzaitanila pa iye masiku onse a moyo wanga . ” Allen , amene tam’chula poyamba nkhani ino , wakhala mu mpingo watsopano kwa caka na miyezi . ( Yer . 20 : 11 ) Mofanana ndi Eliya , mwina ndinu wokhumudwa cifukwa utumiki wanu ukuoneka kuti subala zipatso kapena cifukwa cakuti mwalephela kukwanilitsa zolinga zanu za kuuzimu . Kodi Yehova anali kumuthandiza bwanji ? Kodi zokamba zanga zimaonetsa kuti nimalaka - laka zinthu zotani ? Baibulo limanena kuti : “ Pa ciyambi , panali wina wochedwa Mau , ndipo Mauyo anali ndi Mulungu . ” Koposa zonse , kacisiyo anali kudzakhala “ nyumba ya Yehova Mulungu woona . ” 10 : 40 - 42 ; 1 Akor . 15 : 6 ) Koma ophunzila ake onse a m’nthawi ya atumwi anazindikila kuti lamulo limenelo linali kuwakhudza ngakhale kuti Yesu sanalankhule kwa io mwacindunji . ( Mac . 8 : 4 ; 1 Pet . Sin’nayembekezele kuti munthu wamba monga ine ningaitanidwe ku Giliyadi . Kodi anthu ambili masiku ano amamvetsela uthenga wabwino m’njila iti ? Tikamayandikila Yehova m’pemphelo , nayenso amatiyandikila . Iye anayankha kuti , “ Cabwino , muzikapeleka zakudya kwa asilikali amene ali kunkhondo . ” Koma ulendo umene Paulo anakambapo unali kufunika kukhalako mu September kapena October . Ngakhale pambuyo pakuti Yesu wamuongolela , Petulo anapitilizabe kulimbana ndi mtima wodzikonda . Komabe , Mkhristuyo afunika kukumbukila kuti ngakhale wapemphedwa kuthandiza ana mwauzimu , iye sindiye kholo la anawo . Yesu anauza Yehova kuti : “ Ndikutamanda inu Atate pamaso pa onse , Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi , cifukwa mwabisila zinthu zimenezi anthu anzelu ndi ozindikila ndipo mwaziulula kwa tiana . Mnzako uzimuweluza mwacilungamo . ” Koma zilibe munda umene zimabyalapo mbewu ndi kukolola zakudya . Ambili amatelo , ndipo ena amalosela za mtsogolo . Kodi dziko lidzaonongedwa ndi ngozi zacilengedwe ? Nili m’ndende mu 1962 Mau a Mulungu amakamba kuti : ‘ Ucimo unaloŵa m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi [ Adamu ] , ndi imfa kudzela mwa ucimo , imfayo n’kufalikila kwa anthu onse . ’ Tingadzipende bwanji kuti tidziŵe ngati timaona ndalama moyenela ? Ndipo anapezelapo mwayi wouza banjalo zambili zokhudza Mboni za Yehova ndiponso anawagaŵila zofalitsa . Baibo imakamba kuti mkazi wacikhristu ‘ amatetezeka mwa kubeleka ana . ’ ( 1 Tim . Tsiku limene Yesu anaukitsidwa , anaonekela kwa ophunzila ake osiyanasiyana nthawi zosacepela zisanu . — Mat . N’nali na luso lokamba mfundo zomveka pomenyela ufulu anthu akuda , koma sizinaphule kanthu . Masiku ano , cikondi ca anthu pa Mulungu cikucepela - cepela . pa udindo wathu ? Ngakhale zinali conco , ndinavomela cifukwa ndinakumbukila mbali yaciŵili ya lemba la pamtima panga limene limati : “ Yehova Ambuye Wamkulu Koposa ndiye pothaŵilapo panga . ” 2 : 16 - 18 . ( Agal . 6 : 7 ) Ngati kuti Yehova amasankha mayeselo amene angatigwele , kodi si ndiye kuti akupondeleza ufulu wathu wosankha ? Kuyelekezela nchito yathu ndi mame , kungatithandizenso kuona kuti khama limene aliyense wa ife amacita mu ulaliki n’lofunika kwambili . M’malo mwake , Yehova amasamalila anthu amene iye adziŵa . Nkhani zimene takambilanazi ziyenela kukuthandizani kukhala na cikhulupililo monga ca Marita . 8 : 22 , 23 , 29 . Tingaonetse bwanji kuti timalemekeza mwininyumba ? Makolo amene ali ndi nzelu zopindulitsa amathandiza ana awo kumvetsetsa cifukwa cake afunika kuwamvela . Kodi tiphunzilapo ciani pa nkhaniyi ? Bruce Metzger analemba kuti : “ Mawu olakwikawo [ a pa 1 Yohane 5 : 7 ] mulibe m’mipukutu yonse yakale ( ya Cisiriya , Cikoputiki , Ciameniya , Ciitiyopiya , Ciarabu , Cisilavo ) , kupatulapo ya Cilatini . ” Mwacitsanzo , timadziŵa zambili zokhudza Satana na misampha yake . Ngakhale n’conco , io anapeza mpingo umene munali acicepele ocepa , koma munali atumiki a pa Beteli ambili . Mu 1999 , n’nabatizika n’kukhala wa Mboni za Yehova . Ndine woyamikila kwambili kuti nilinso na mwayi wokhala ndi umoyo wabwino ndi wacimwemwe . Popeza kuti timadziŵika ndi dzina la Yehova , zocita zathu zimakhudza mmene ena amaonela dzina lake . ( Maliko 13 : 9 ) Mau amenewa aonetsa kuti Akristu adzakumana ndi masautso acindunji monga cizunzo . Nthawi zina atsogoleli acipembedzo kapena andale angacititse kuti tizunzidwe . ( Mac . Mwanzelu , Davide anapempha Yehova kuti “ mundiletse kucita modzikuza . ” ( Sal . Nikodemo , amene anali membala wa Khoti Yapamwamba ya Ayuda , anacita cidwi ndi zimene Yesu anali kuphunzitsa . 35 : 30 . ( Aheberi 12 : 1 ) Mofanana ndi Petulo , nafenso ngati tiganizila kwambili zinthu zoipa , cikhulupililo cathu cingayambe kufooka . 7 : 9 , 10 ) Cotelo , kudzipeleka na kubatizika n’zofunika ngako . Kuwonjezela apo , sadzakhala na moyo kwamuyaya . ( Aroma 15 : 4 ) Pamene tisinkhasinkha zitsanzo zawo , tingacite bwino kuganizila kutalika kwa nthawi imene anafunika kuyembekezela , cifukwa cake anali wokonzeka kuyembekezela , komanso madalitso amene anapeza cifukwa ca kuleza mtima kwawo . Ufumu wa Mulungu ndi boma la kumwamba . Nkhani iyi idzafotokoza lemba lathu la caka ca 2018 , ndipo ionetsa cifukwa cake timafunika kudalila Yehova kuti atipatse mphamvu . M’nkhani yotsatila tidzakambitsilana mafunso amenewa . Komabe , khalani na cikhulupililo cakuti Mulungu adzakuthandizani kupilila mavuto aliwonse amene mungakumane nawo . Baibo imakamba kuti iye “ amapeleka mphamvu kwa munthu wotopa , ndipo wofooka amam’patsa nyonga zoculuka . ” ( Yes . 40 : 29 ; Sal . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Musamatengele nzelu za nthawi ino , koma sandulikani mwa kusintha maganizo anu . ” — Aroma 12 : 2 . Patapita zaka zopitilila 30 , mtumwi Yohane analemba buku ya Uthenga Wabwino ndi makalata atatu . Mulungu amafuna kuti ‘ tizipempha mogwilizana ndi cifunilo cake ’ zinthu zimene amavomeleza . Conco , musaope olo pang’ono pamene Satana akuwopsezani kuti mugonje . — 1 Pet . Akristu amene ali m’madela amenewo amafunika kuphunzitsa maganizo ao ndi cikumbumtima cao kuti azicita zinthu mwanzelu ngati pabuka mikangano pakati pa mitundu yosiyana . Nkhaniyi ionetsa zimene takhala tikugwilitsila nchito polalikila uthenga wabwino m’zaka 100 za ulamulilo wa Ufumu . N’cifukwa Ciani Tifunika Kutamanda Yehova ? Iye ali ndi mtima woyamikila ndipo amakonda kuganizila zinthu zimene ali nazo . Timaonetsanso kuti timathandiza abale a Kristu mwa kumvela mokhulupilika akulu ndi abale ena oikidwa ndi “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” — Mat . Zinatheka bwanji kuti kuuka kwa Yesu kucitike “ malinga ndi Malemba ” ? Panafunika ndalama zambili kuti tikwanitse kuyenda maulendo onsewo ocoka ku Tokmok kupita ku Balykchy . Koma patapita nthawi , Paulo anazindikila kuti Maliko anakhala wakhama ndi kuti akanatha kumuthandiza pa utumiki wake . Yehova Mulungu wakonza kale za kutipululumutsa kwa mdani ameneyu imfa . Ndipo njila yaikulu imene adzagwilitsila nchito potipulumutsa ndi Yesu Kristu . Nanga ndi zosankha ziti zimene zidzakucititsani kukhala wacimwemwe ? Onani zimene anacita atayamba kukaikila ndi kumila pa nyanja . Baibo imati : “ Zolingalila sizikwanilitsidwa ngati anthu sakambilana moona mtima . ” — Miyambo 15 : 22 . M’maiko ena , anthu ambili alibe cidwi , ndipo ena ni otsutsa . ( Mlal . 7 : 12 ; Luka 12 : 15 ) Nthawi zambili , anthu amene amapita kukafunafuna ndalama ku maiko ena samazindikila kuti pali zambili zimene amafunikila kucita . KWA zaka zambili , Ayuda popeleka pemphelo lawo lapadela , akhala akuchula mau amene ali pa Deuteronomo 6 : 4 . Pokambilana ndi anthu , tingaloŵetsemo bwanji lemba la Mateyu 5 : 3 ? “ Nimakonda kukhala na zolinga . ( Yobu 34 : 10 ) Mulungu si amene acititsa zoipa kapena mavuto amene tiona padziko . M’madela ambili padziko lapansi , anthu amagwilizana kwambili cifukwa cokhala ndi mbili yofanana , cikhalidwe ndi cinenelo cofanana ndipo zimenezi amazinyadila . Mbonizo zinationetsa m’Baibulo pofuna kutitsimikizila kuti Akristu oona salambila mafano , ndi kuti mapemphelo ayenela kupelekedwa kwa Mulungu yekha . Angelo anathandiza Yesu . Komanso , anthu oipa angasonkhezele ena kucita zoipa , ndipo akatelo amaonjezela zinthu zoipa . — Miyambo 1 : 10 - 16 . Mbali yoyamba imene anthu ambili akulimbana nayo ni zofooka zathupi . ( Mateyu 5 : 16 ) Conco Akristu oona tingawadziŵe cifukwa ca cikondi cimene amaonetsa kwa anansi ao powacezela n’colinga cowauza uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . — Ŵelengani Mateyu 24 : 14 ; Machitidwe 5 : 42 ; 20 : 20 . Kodi ndi gulu liti limene limalalikila uthenga umenewo kwa anthu onse ? Iye anati : “ Koma ine ndidzadikilila Yehova . Tikamadziunjikila “ cuma padziko lapansi , ” timakhala ndi nkhawa kwambili . ( Mat . Zimenezi zimaonetsa kuti lonjezo limene Yesu ananena lokhudza kuika patsogolo Ufumu ndi loona . Zimene zinacitika pambuyo pake zinalimbitsa cikhulupililo ca Gidiyoni ndipo anayandikila kwambili kwa Yehova . Mwanjila imeneyi , opatsa ndi olandila , onse ali na mwayi wokhala mabwenzi a Yehova . Mwina nthawi yothela imene munaonana ndi munthuyo munasiyana maganizo . ( b ) Kodi panakhala zotulukapo zanji pamene Mboni ina ya ku Austria inaonetsa ulemu kwa mtsogoleli wina wandale ? Yesu anali kumva cisoni cimene anthu ena anali naco ndipo anali kukondwela ndi anthu amene anali kukondwela . Pamene anali padziko lapansi , nkhani imene anali kukamba nthawi zambili inali yonena za Ufumu wa Mulungu . Kodi malangizo a pa Aefeso 4 : 23 , 24 akukhudza ndani ? Ndipo Hananiya na mkazi wake Safira anafa cifukwa conama . Ise sitifuna kutengela anthu amenewa . Ngati tili paubwenzi wabwino na Yehova , iye adzatikhululukila , adzatithandiza kucila mwauzimu , ndi kutipatsa mphamvu kuti tisagonje ngati tayesedwanso kuti ticite chimo . — Sal . Blessing atacotsedwa m’dziko lina la ku Europe , anapita ku Spain . N’zokondweletsa kuona kuti anthu ambili akumvetsela uthenga wabwino wa Ufumu . Tikuyembekeza mwacidwi nthawi imene Mulungu adzakwanilitsa lonjezo lake lakuti : ‘ Padziko lapansi padzakhala tiligu wambili . ’ “ Mulungu amene amaona ciliconse ” amakuonani inunso . Colinga cake cinali “ kucitila umboni mokwanila ” mosasamala kanthu ndi mazunzo . Tiyenela kutengela citsanzo ca ophunzila a Yesu odzicepetsa . Kuti akwanilitse colinga cake , mu June 1523 , anafalitsa Mabaibo a Uthenga Wabwino , voliyumu 1 ndi voliyumu 2 m’Cifulenchi . Mwina munavutikapo cifukwa ca tsankhu ndi kupanda cilungamo . Koma pamene mngelo anauza Danieli kuti ‘ adzauka kuti alandile gawo lake , ’ anaonetselatu kuti Danieli adzaukitsidwa pa ciukililo cam’tsogolo cimene cinali kudzacitika zaka zambili pambuyo pa imfa yake . Mlongo wina anali kupita kunyumba yosungila okalamba kukaona amai ake pafupi - fupi tsiku lililonse . Mwacitsanzo , ndani amaona nchito yoonkhetsa ndalama ndi kudzaza mapepala a maakaunti imene mtumiki wa maakaunti amacita mwezi ulionse ? Magazini ya Watch Tower inalimbikitsa kuti : “ Bwelani pokhala kuti mitima yanu ndi yosefukila ndi cikondi ca Ambuye , ca abale ake , ndi coonadi cake . ” ( Mateyu 26 : 38 ) Ngakhale kuti zocita zao sizinam’kondweletse , Yesu sanaleke kulankhula ndi mabwenzi ake . — Mateyu 26 : 40 , 41 . ( b ) N’cifukwa ciani na imwe muona kuti mufunika kukhala woleza mtima na mwana wanu ? Kufunafuna Cuma Ceni - ceni , July “ Mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa ” unaonetsa kuti Mulungu anali ndi ufulu wosiyanitsa cabwino ndi coipa . Iye amakhala wofunitsitsa kwambili kulandila thandizo la kuuzimu limenelo ndi kuligwilitsila nchito . — Miy . 8 : 44 ) Conco , olo kuti ndise opanda ungwilo , tifunika kuyesetsa kupewa kunama . ( Aef . Ganizilani izi : M’mipingo yathu masiku ano , muli akazi acikulile okhulupilika monga Debora , acinyamata anzelu monga Elihu amene akutumikila monga akulu , apainiya olimba mtima ndipo acangu ngati Yefita , ndiponso amuna ndi akazi okhulupilika ndipo oleza mtima monga Yobu . Conco , Akhiristu sayenela kuwonjezelaponso nkhawa zina poganizila kwambili za mavuto akumbuyo kapena akutsogolo . 8 , 9 . ( a ) N’ciani cingatithandize kukhala okhazikika m’cikhulupililo ? 1 : 11 . Anthuwo anaona kuti kukambitsilana pasadakhale mwacikondi ndi mokoma mtima kunaŵathandiza kupanga zosankha popanda mavuto . “ Ndikuganizila zokupatsani mtendele osati masoka , kuti mukhale ndi ciyembekezo cabwino ndiponso tsogolo labwino . ” — Yeremiya 29 : 11 . Ngati tiseŵenzetsa bwino malamulo na mfundo za m’Mau a Mulungu , tikhoza kukhala “ woyenelela bwino ndi wokonzeka mokwanila kucita nchito iliyonse yabwino . ” ( 2 Tim . Kodi Yehova wakhala akulamulila motani anthu kucokela pa kupanduka kwa m’munda wa Edeni ? NYIMBO : 152 , 22 Kwa zaka zambili , ulamulilo wa Yehova unatsutsidwa kumwamba ndi padziko lapansi . Kucita zimenezi kumangoonetsa kuti womwalilayo mumam’kumbukila ndi kuti mumam’konda kwambili . Mungatambe vidiyo yosimba za umoyo wake imene ili pa JW Broadcasting . Cilamulo cinakamba kuti zonyansa za munthu ziyenela kufoceledwa kutali . ( b ) N’ciani cinathandiza Yosefe kusangonja pamene mkazi wa Potifara anali kumunyengelela ? Pa cifukwa cimeneci , sitikuopa kukumananso ndi mavuto azacuma . Seth Hyatt 65 : 2 . Pofuna kuthandiza anthu ambili kuphunzila coonadi , ndinayamba upainiya . “ Taganizilani za cikondi cacikulu cimene Atate watisonyeza . ” — 1 YOHANE 3 : 1 . Koma tiyeni titengele citsanzo ca Gidiyoni ndi asilikali ake . Coyamba iwo anayenda kudziko la Harana , pa mtunda wa makilomita 960 kumpoto ca kum’madzulo , motsatila mtsinje wa Firate . Kodi cikumbumtima cathu cingatithandize bwanji kupanga zosankha zanzelu ? Wolemba Salimo 147 anasonkhezeleka kutamanda Yehova . ( Mac . 2 : 11 , 41 ) Atakula , Kristina anakambilana nkhaniyi ndi makolo ake , ndipo anaganiza zosamukila mumpingo wa citundu ca kumaloko . ( a ) Kodi Yehova anam’lonjeza ciani Davide ? Mu 1530 , Baibo imene anatsiliza kumasulila inapulintiwa kunja kwa dziko la France , mumzinda wa Antwerp , movomelezedwa ndi Mfumu Charles Wacisanu . Amadelanso nkhawa cifukwa ca mavuto amene amabwela ndi ukalamba . N’tagwila nchito kwa zaka ziŵili , n’nafunsanso woyang’anila dela wina za upainiya . M’malo moyankha funso limenelo mwacindunji , Yehova anatsimikizila mneneli wake wokhulupilikayo kuti cionongeko cimene anakambilatu ‘ sicidzacedwa . ’ Nanga ndimalankhula molimba mtima za cikhulupililo canga ? Kumbali ina , anthu ena amapemphela kwa Mulungu kokha akakumana ndi mavuto , ndipo amayembekezela kuti pempho lao liyankhidwe pamenepo . — Yesaya 26 : 16 . Ena angafunse kuti : ‘ Kodi Mulungu sangaletse zinthu zoipa zimenezi kuti zisacitike ? “ Pitilizani . . . kukhululukilana ndi mtima wonse . ” — AKOLOSE 3 : 13 . “ All Scripture Is Inspired of God and Beneficial ” — Buku limeneli lili na mfundo zimene zinafufuzidwa mosamala . Limafotokoza nthawi na malo kumene mabuku a m’Baibo analembedwela ndiponso cifukwa cake buku lililonse linalembedwa . Iye anati : “ Panthawiyo , ine , mwamuna wanga , ndi mlongosi wanga tinali kuthedwa nzelu . Iye anati : “ Inde , ni wabwino ngako . Ni kudalila kwambili Yehova osati mphamvu zathu , komanso kukhulupilila dipo , monga mmene Paulo anacitila . Kodi mtumwi Paulo anakamba ciani pa nkhani ya kulimbikitsana ? M’nkhani ino , tidzaphunzila zitsanzo zakale ndi zamakono za anthu amene atumikila Yehova . Ngati tiona kuti nzelu zocokela kwa Yehova n’zofunika kwambili , tidzakhala wofunitsitsa kudzaza mosungila cuma cathu mfundo zatsopano ndi zakale za coonadi . Komabe , popeza ndife opanda ungwilo n’zosatheka kupewa matenda onse . Kanali koyamba kugwilako nchitoyo , koma abale anadzipeleka kuti anithandize . Kuganizila madalitso amenewo kunalimbitsa cikhulupililo cao mwa Yehova . — Ŵelengani Aheberi 11 : 15 , 16 . Koma posakhalitsa , cisangalalo cao cinatha ndipo anakhumudwa ndi zimene zinacitika . Nthawi imafika pamene okalamba sangathenso kudzisamalila , ndipo amafuna thandizo . Iye anati : “ Nidziŵa kuti ni Ufumu wa Mulungu cabe umene udzacotsapo mavuto athu onse . ” Magulu aŵili a asilikali , la Afilisiti ndi la Aisiraeli , anangokhala cilili osacita ciliconse pamene Goliyati anali kunyoza Aisiraeli tsiku na tsiku . ZOTSATILAPO ZAKE : Mipukutu ya Baibulo masauzande ambili ikalipo . 3 : 28 ; 6 : 15 , 16 ) Pakati pa akazi Acikristu amene anali kulalikila m’nthawi ya atumwi , panali ana aakazi anai a mlaliki Filipo . — Mac . 21 : 8 , 9 . Koma Yesu analimbikitsa otsatila ake kuti afunika kudzipezela mabwenzi kumwamba ndi zolinga zabwino . Acifwamba amene anakumana nao pa njila anali kuimila mabungwe akuluakulu komanso amalonda adyela , ndipo wansembe ndi Mlevi anali kuimila machalichi acikristu . Pambuyo poyelekezela Mabaibulowo ndi mipukutuyo , akatswili amenewo anapeza mavesi oŵelengeka cabe amene anali osiyanako pang’ono . Koma Baibulo limati : “ Amene amacita dama amacimwila thupi lake . ” Atangophunzilako kamodzi , mkazi wanga analeka kukoka fodya , anayamba kukana kutenga ndalama zakuba , ndipo anandibwezela ndolo ( masikiyo ) , mphete , ndi zibangili . Malinga n’zimene Malaki analemba , kodi Yehova amawaona bwanji anthu amene amam’tumikila na mtima wonse ? Koma a “ nkhosa zina ” adzalandila moyo wosatha padziko lapansi mmene “ mudzakhala cilungamo . ” ( Yoh . 10 : 16 ; 2 Pet . Ndiyeno , Yesu anafotokoza zimene zidzacitikila anthu amene amalephela kucita cifunilo ca Yehova zinthu zikafika poipa . Anthu a m’banja limenelo anali okoma mtima , koma anali kungotengela zocita za anthu ambili a pa nthawiyo . Kudzipeleka ni lonjezo lakuti tidzayamba kukonda Mulungu na kuika cifunilo cake patsogolo kuposa cina ciliconse . 9 : 23 , 24 ) Ngati tisunga maganizo oipa mumtima mwathu , m’kupita kwa nthawi adzaonekela m’kacitidwe kathu ka zinthu . Komanso , posacedwapa anthu ena ku South Africa aona makhalidwe abwino amene anthu a Mulungu ali nawo . “ Zinthu zimene unazimva kwa ine . . . , uziphunzitse kwa anthu okhulupilika . ” — 2 TIM . ( Aef . 6 : 4 ) M’nkhani ino , tidzakambilana zinthu zitatu zimene makolo angacite kuti akhale abusa a kuuzimu a ana ao . Koma kodi pali umboni uliwonse woonetsa kuti lonjezo lakuti akufa adzauka lingakwanilitsidwe ngakhale patapita zaka zambili ? Nthawi zina , mungade nkhawa na zimene zikukucitikilani . ( Deuteronomo 28 : 58 - 61 ) Panthawi ina , Yehova anateteza anthu ake ku matenda . Tikafunsa mwininyumba funso , kodi tiyenela kucita ciani ? Masiku ano , Akristu odzozedwa amacitanso utumiki umenewu . Paulo anapempha anzake kuti : “ Inunso mungathandizepo mwa kutipelekela mapembedzelo anu . ” Baibo imati : “ Dziko likupita limodzi ndi cilakolako cake , koma wocita cifunilo ca Mulungu adzakhala kosatha . ” Tonse timafunika kupanga zosankha mwanzelu . Maiyo anali waubwenzi ndipo anauza mlongoyo kuti : “ Loŵani . Rosario mmodzi wa akatswili amene anali kumuthandiza kulankhula anati : “ Nditafuna kumapemphela , ndingakhale mmodzi wa Mboni za Yehova . Atalalikila kwa miyezi iŵili , anakumana ndi mai wina amene anali kulela yekha mwana . Ndikuika kuti udziyang’anila zinthu zambili . ” Iye anati : “ Pamisonkhano , tinaphunzila Nsanja ya Mlonda ndi kuimba nyimbo za Ufumu . Ndipo sindikukaikila ngakhale pang’ono kuti Yehova adzaukitsa mwamuna wanga . ” — Afil . Pa April 16 , 1922 , M’bale Rutherford anakamba nkhani yake yoyamba ya pa wailesi , ndipo anthu pafupifupi 50,000 anamvetsela . Ndipo ndi mtima wathu wonse , tiyeni tinene mofanana ndi wamasalimo kuti : “ Cipulumutso cimacokela kwa Yehova . Mau a Paulo palembali amaonetselatu kuti zimakhala zovuta kuti munthu wauzimu akhale ogwilizana na munthu wakuthupi . Abale na alongo ena otumikila ku malo osoŵa anadzionela okha mphamvu ya pemphelo . Mbali yothela ya lemba la Yohane 3 : 16 limafotokoza zimene Mulungu walonjeza anthu amene amakhulupilila nsembe ya dipo ndi kutsatila miyezo ya Mulungu paumoyo wao . Iye anadziŵa kuti nthawi yake yotumikila idzatha , ndipo ena adzafunika kupitiliza ndi nchitoyo . ( Luka 11 : 3 ) Nkhani za m’Baibulo zimaonetsa kuti Yehova akhoza kutipatsa ciliconse cimene tifuna . N’ciani cimakukondweletsani na kalamulidwe ka Yehova ? Koma kukhululuka ni cosankha cimene munthu amapanga pambuyo poganizilapo bwino . Zimenezi zimaonetsa kuti ni wokonda mtendele ndipo afuna ubwenzi wake na munthu amene wamulakwila upitilile . 21 : 20 , 21 , 27 - 29 ; 2 Maf . 20 : 1 - 5 ) Tingadziŵenso mfundo zina zimene zingatipangitse kuona kuti ndi bwino kusintha zimene tinasankha . Ndipo nthawi iliyonse imene walimbikitsa mpingo mwa njila imeneyi , amamwetulila kwambili . Kodi mumakondwela pamene muŵelenga Baibo kapena simukondwela ? Anali kutumikila Mulungu amene sasintha , ndiponso amene ni wokhulupilika nthawi zonse . Ngati tidalila citsogozo ca Yehova na kutsatila mfundo zimene watipatsa , tidzatha kupanga zosankha mwanzelu ndipo sitidzakhala wokayika - kayika pa zocita zathu . — Yak . 4 : 9 , 10 . Pokamba za Mwana wokondedwa wa Yehova , Paulo anati : “ Kudzela mwa iyeyu [ Yesu ] tinamasulidwa ndi dipo la magazi ake , inde , takhululukidwa macimo athu , malinga ndi cuma ca kukoma mtima kwake kwakukulu [ kwa Yehova ] . ” Junia , amene m’bale wake anadzipha , anakamba kuti : “ Ngakhale kuti simungamvetsetse zonse zokhudza cisoni cimene munthu wofedwa ali naco , cofunika ngako ni nkhawa imene mwamuonetsa mwa kuyesetsa kumumvetsela . ” Mofananamo , ngati tifuna kuti Yehova atithandize kupilila , sitiyenela kutaya mtima koma tiyenela kutsatilabe mfundo zake za m’Baibulo . 5 : 8 ) Satana angagwilitsile nchito njila iliyonse kuti aticititse kukhala osakhulupilika kwa Mulungu . Kupendanso mau a Paulo a pa 1 Akorinto 10 : 13 , kwatifikitsa pa mfundo iyi : Palibe cifukwa ca m’Malemba cokhulupilila kuti Yehova amadziŵilatu mayeselo amene tingakwanitse kuwapilila , ndiyeno malinga na zimene waona , n’kusankha mayeselo amene tingakumane nawo . Tsiku limenelo n’losaiwalika kwa ine . Mofanana ndi zimene Yehova anauza Aisiraeli akale , iye awagwila dzanja lamanja ndi kuwauza kuti : “ Usacite mantha , pakuti ndili nawe . ” — Yes . Kodi anthu odzitukumula na onyada amadziona bwanji ? ( Ŵelengani Genesis 3 : 15 . ) Amati iwo akalapa moona mtima , anali kuwaonetsa cikondi ndi cifundo cake , pokamba kuti : “ Ndidzathetsa kusakhulupilika kwawo . Anakambanso kuti : “ Poyamba , kucita zaciwelewele kunali kunipangitsa kudziona kuti ndine wofunika , ndi kuona kuti anthu ena amanikonda . 13 : 12 ) M’nthawi zakale , kukhala wosabala cinali cinthu cocititsa manyazi . 8 , 9 . ( a ) Kodi pamakhala kusintha kotani ngati kholo likhala kutali ndi banja lake ? 31 : 5 ) Mwa ici , iye amafuna kuti “ aliyense wa ” olambila ake ‘ azilankhula zoona kwa mnzake ’ ndi kupewa ‘ kunama . ’ ( Aef . 4 : 25 ; Akol . Sindinali kuganizila zokhala pa cibwenzi ndi m’bale Atsushi , ndipo sindinaganizilepo kuti angandifune . Mgwilizano wa Zipembedzo — Kodi Mulungu Amauvomeleza ? Zonsezi zinathandiza kuti tizikondana kwambili ndi abale na alongo a m’dzikolo . Mkristu mnzathu angafunike kulimbitsa cikhulupililo cake mwa kukhala ndi phunzilo laumwini , kupemphela , ndi kucita zinthu zina za kuuzimu . Ndipo timaona kuti kukhulupilila Yesu n’kofunika kuti munthu apulumuke . Conco , n’tabatizika pa msonkhano wacigawo wa ku Toronto , n’nasaina fomu yofunsila utumiki wa pa Beteli . ( Luka 2 : 22 - 24 ) Pamene Mariya anali kupita ku kacisi pamodzi na Yosefe komanso Yesu , mwina anali kuganiza kuti akafika kumeneko , wansembe adzakamba mau ena ake oonetsa kuti anali kudziŵa udindo umene Yesu adzakhala nawo m’tsogolo . Mudzakondwela kwambili kuona ana anu akusankha kutumikila Mulungu ndi kupitilizabe kum’tumikila mokhulupilika . — 3 Yohane 4 . Aka n’kamvedwe katsopano . Popeza kuti Mkristu akacotsedwa mumpingo cimapweteka kwambili , n’cifukwa ciani tinganene kuti amenewa ndi makonzedwe acikondi ? Siniona kuti n’nalakwitsa kupita kulikonse kumene Ambuye ananituma . Iye anali kucilitsa anthu nthawi yomweyo , ndipo nthawi zina anali kucilitsa ngakhale anthu amene anali kutali . ( Yoh . ( Aefeso 1 : 18 ) Tiyeni tione njila zitatu zimene zingatithandize kucita zimenezi . 12 : 25 ) Izi zimacitikila aliyense wa ise . ( Aheberi 11 : 11 ) Sara anali kum’dziŵa Yehova , anali kudziŵa kuti angakwanilitse lonjezo lililonse . Olo kuti anali na zaka pafupi - fupi 80 , iye anaonabe kuti afunika kubatizika . “ Kodi Ndingatani Kuti Ndikhale Paubwenzi ndi Mulungu ? ” — mutu 35 Ngati Adamu sanadye cipatso cimeneci , akanaonetsa kuti akumvela Mlengi wake komanso kuti akumuyamikila kaamba ka zinthu zoculuka zimene anam’patsa . Coyamba , anafunsila malangizo kwa amuna acikulile amene anali alangizi a Solomo , atate wake . N’ciani cidzayamba kucitika makhalidwe oipa akadzatha ? Mungacitenge m’nkhani zakuti “ Baibulo Imasintha Anthu ” mu Nsanja ya Mlonda . 22 : 7 ) Satana amafuna kuti tiziwononga nthawi yathu ndi mphamvu zathu zonse pocilikiza dongosolo la zamalonda la m’dzikoli . N’zoona kuti Mulungu amatha kudziŵilatu zamtsogolo . Koma funso limene tifunika kuganizila ndi ili : Kodi Mulungu amaonetsa mphamvu zake zimenezi zodziŵilatu zinthu zamtsogolo popanda malile ? — Yesaya 42 : 9 . Tikatsiliza kulalikila m’gawo lonse , tinali kupita m’tauni ina . ” Komabe , kodi Mulungu amagwilitsila nchito bwanji zimene amadziŵa zokhudza inu kuti akuthandizeni ? [ Cithunzi papeji 5 ] ( Miyambo 10 : 22 ; 1 Petulo 5 : 8 ) N’cifukwa cake makolo acikristu ayenela kupeza nthawi yophunzitsa ana ao tanthauzo la kukhala wophunzila wa Kristu . Popeza kuti cikondi canga coyamba kwa Yehova cinali camphamvu kwambili , ndinali kuwalalikila mopanda mantha koma mosasamala . Mwamwayi , mu 1941 , asilikali a Britain ndi a mayiko ena analoŵa m’dziko la Greece , ndipo Nicolas anatulutsidwa m’ndende . Conco , iwo anadzifunsa kuti , ‘ Ngati helo ni malo ozunzilako anthu oipa , n’cifukwa ciani Yesu anapita kumeneko ? ’ Iye anali kulalikila mwakhama kwambili , ndipo anayenda m’madela ambili monga ku Siriya , Asia Minor , Makedoniya , ndi Yudeya . Nidzamuuza za vuto lako . M’nkhani yoyamba , tidzakambilana tanthauzo la kukhala munthu wauzimu komanso zimene tingaphunzile pa zitsanzo za anthu auzimu . Koma cokondweletsa n’cakuti anthu ambili amadzipeleka kuti asamalile munthu amene amakonda yemwe akudwala matenda osacilitsika . Maganizo amenewa ni ofala cakuti ambili amaona kuti kukhala osaona mtima ndiyo njila yabwino yopezela cuma . Makolo oopa Mulungu amapewa kungotengela cikhalidwe cakwawo colelela ana . KUONONGEDWA KWA MZINDA WAUKULU : Mwacitsanzo , kulosela ndendende kuti mzinda waukulu , umene kwa nthawi yaitali unali wolimba udzaonongedwa cinali cinthu cocititsa cidwi . Kodi ana ena angathandizileko mbali zina , monga kusinthana - sinthana kupeleka cisamalilo ? Cifukwa ca khalidwe loipa la Yehoyakimu , Yeremiya analosela kuti : “ Adzaikidwa m’manda ngati mmene amaikila bulu wamphongo . ” Makope amene tili nawo ali ndi zolakwika zambili , ndipo analembedwa zaka mahandiledi ambili mipukutu yoyambilila ya Baibulo italembedwa kale . Makope amenewa ni osiyana ndi mipukutu yoyambilila m’njila zambili . ” Petulo anapempha Yesu kuti amulole kuyenda pamadzi kupita kwa iye . N’ciani cimene mwamuna ayenela kucita kuti mkazi wake azim’konda ndi kumulemekeza ? Ndikuyamikila kwambili Yehova komanso inuyo . ” Pakali pano taphunzila Baibo ndi anthu a Cichaina okwana 112 . Gener anali kufika panyumba usiku pambuyo poseŵela maseŵela ena ocedwa billiard ndiponso maseŵela aciwawa a pa kompyuta ndi anzake . Yesu anakamba kuti ophunzila ake oona ndi amene adzagwila nchito imeneyi . A Zulu : Onaninso zimene ulosi ukunena : “ Ulamulilo wake udzakhalapo mpaka kalekale ndipo sudzatha . Ufumu wake sudzawonongedwa . ” Kodi tidzakhalabe oona mtima ngati tiona kuti tingapeze cuma mwa kukamba bodza ? ( b ) Ndi kukambitsilana kwina kuti kumene inu mwapeza kuti n’kothandiza pankhani yopita kumwamba ? Iye akatiphunzitsa njila zake , ndipo ife tidzayenda m’njila zakezo . ’ Nanga ndingapulumuke bwanji ? Cikondi ca Yehova pa anthu cili monga cikondi ca makolo pa ana awo . Koma Sara sanacite zimenezo . Mkhristu aliyense ayenela kukhala wobatizika , ndipo ubatizo ni wofunika kuti munthu akapulumuke . — Mat . Conco , tikadziŵa mmene tingagwilitsile nchito kapepala kamodzi , ndiye kuti tadziŵa tonse . Kodi zimene Petulo anakamba zakuti ubatizo ufanana ndi cingalawa zitiphunzitsa ciani ? Mwacionekele , Kristu adzasankha ena mwa akulu okhulupilika amene tili nao masiku ano kuti akatitsogolele m’dziko latsopano . — Yes . Japan 220,000 Kuukila mwakabisila kwa Satana kusiyana bwanji ndi kuukila mwacindunji ? Kuonjezela pamenepo , Yesu anauza otsatila ake kuti : “ Mukaphunzitse anthu a mitundu yonse . ” ( Mat . Pa nthawiyo , anthu anali otangwanika ndi zocitika za umoyo wa tsiku ndi tsiku , kuphatikizapo kukwatila ndi kukwatiwa . Mwa ici , anthuwo sanasamale na zimene “ Nowa , mlaliki wa chilungamo , ” anali kuwacenjeza za ciwonongeko cimene cinali kubwela . ( 2 Pet . ( Salimo 65 : 2 ) N’cifukwa cake Yesu anauza ophunzila ake kuti , “ azipemphela nthawi zonse , osaleka . ” Khalidwe la kuleza mtima tidzalikambilana m’tsogolo , m’nkhani ina yofotokoza “ cipatso ca mzimu . ” Inganithandize bwanji pa mavuto amene nimakumana nawo ? ’ “ Pali umboni wosatsutsika woonetsa kuti mlengalenga wa padziko lapansi , nyanja , ndiponso mtunda zikutentha kwambili . . . ( b ) misonkhano ya mpingo ? Pikica yoonetsa anthu ogwidwa ukapolo ku Iguputo wakale Donald Gordon Patangopita nthawi yocepa , Yehova analonjeza Abulahamu kuti adzam’patsa zoculuka kuposa zimene analuza . ( 2 Pet . 1 : 7 ) N’zoona kuti sitiyenela kukakamizika kuthela nthawi yambili mu ulaliki kuti tizipeleka maola ambili . Zipembedzo zambili zimakhulupilila kuti kuli zolengedwa zauzimu zamphamvu , zimene amati n’zacifundo , ndipo zimacita cifunilo ca Mulungu na kuteteza anthu . Nanga bwanji chechi yanu ? ( b ) Kodi zinthu zinali bwanji pamene Ezekieli analemba mau a pa Ezekieli 14 : 14 ? Koma kuti cikumbumtima cizititsogolela bwino , tifunika kuciphunzitsa . Popeza ndise anthu opanda ungwilo , nthawi zina tingacite zinthu zokhumudwitsa Yehova . Dipo imapambana mphatso zonse . Iyo inali na mafunso ambili okhudza Baibo . Ni malangizo ati amene tinapatsidwa okhudza maphunzilo athu a Baibo ? Ngati tipitiliza kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova , iye adzakhala Bwenzi lathu mpaka kalekale Palibe munthu aliyense padziko lapansi amene adziŵa tsiku limene Ufumu wa Mulungu udzabwela . — Mateyu 24 : 36 . Mucititseni kudzimva kuti akhoza kukondweletsa inu ndi Yehova ndi kuti angagwilitse nchito maluso ake potumikila Yehova . N’cifukwa ciani Yehova ndiye woyenela kulamulila cilengedwe conse ? Sadie Green anali mmodzi wa odzipelekawo . Tikamaphunzila Baibulo , colinga cathu n’cakuti tim’dziŵe bwino Yehova . Nanga ningacite ciani kuti niziimba na mtima wonse ? ’ Markin ) , May Pokamba za Atate wake , Yesu anati : “ Nthambi iliyonse mwa ine yosabala zipatso amaidula . ” Pamene anali akapolo ku Iguputo anapanga nchelwa zambili moti sanafune kukumbukila za nchitoyo cifukwa inali yaukapolo . Banja loyambalo linali ndi mwayi wogwila nchito yokhutilitsa , yosangalatsa , komanso kutulukila zinthu zatsopano kwamuyaya . Kodi cinacitika n’ciani kuti anthu ayambe kufa ? Mofananamo , munthu mmodzi sangathe kulalikila anthu onse padziko lapansi . Koma pokambilana ndi ophunzila ake , iye sanaonetsa kuti anali wokhumudwa kapena wowawidwa mtima ngakhale pang’ono . Yehova anali kufuna kuti iwo abwelele kwa iye , na kuti apitilize kumulambila na mtima wonse komanso mopanda mantha . Kodi abale na alongo amene akutumikila ku Turkey anakamba ciani cokhudza umoyo wawo kumeneko ? ( Yesaya 30 : 20 , 21 ) Ngakhale anthu ena amene satumikila Yehova , akabwela kumisonkhano yathu , amadziŵa kuti mzimu wa Mulungu umatitsogolela . Analinso ngati tate wawo kuuzimu . — Ŵelengani 1 Atesalonika 2 : 7 , 11 , 12 . 1,003 Ndi zitsanzo ziti zimene zingatithandize kulimbitsa cikhulupililo cathu ? Ngakhale ndi conco , io amadziwa bwino malangizo a mtumwi Paulo okhudza kukwatiwa “ mwa Ambuye . ” Ndipo mwanayo akabadwa , iwo amafunikanso kusintha zinthu zina n’zina paumoyo wawo . Vuto loyamba linali lakuti , Kingsley anali kukhala kunyumba zosungila okalamba ndi olemala . Monga mmene kudya cakudya copatsa thanzi kumalimbitsila thupi , kuphunzila kaganizidwe ka Khristu kumalimbitsa uzimu wathu . Takamba conco cifukwa kalelo “ akazi analandila akufa awo amene anauka kwa akufa , ” koma pambuyo pake anafanso . — Aheb . ( 2 Mbiri 34 : 14 ) Yehova atapatsa Mose malangizo a mmene angapangile cihema , “ Mose anacita zonse monga mmene Yehova anamulamulila . Cioneka kuti , kwa akazi ena , ma IUD amenewa amawalepheletsa kutulutsa mazila . ( Sal . 18 : 25 ) Nkhani yotsatila idzafotokoza zifukwa zina zimene mufunika kucilikizila ulamulilo wa Yehova na mtima wonse komanso mmene mungacitile zimenezi . 3 : 8 ) Komabe , izi sizitanthauza kuti ngati Mkhristu amamwa pa mlingo woyenela , ndiye kuti basi zonse zili bwino . Potengela citsanzo ca m’Baibulo cimeneci , Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova lapanga masinthidwe okhudza kuika akulu ndi atumiki othandiza pa udindo . Paulo asanakhale Mkhristu , anali wamkali ndi woopsa . Izi zingapangitse kuti mimba imene inakhala , ipitilile . Kukhala ndi maganizo amenewa kumakwanilitsa ulosi umene uli pa Salimo 110 : 3 . Ngakhale n’conco , Yehova amayesetsabe kutithandiza . Yehova watiphunzitsa “ kukana moyo wosaopa Mulungu ndi zilakolako za dziko , koma kukhala amaganizo abwino , acilungamo ndi odzipeleka kwa Mulungu m’nthawi ino . ” Kodi tiyenela kutsimikiza mtima kucita ciani ? Ndipo n’cifukwa ciani ? Kodi anthu ena m’dela lanu “ cikhulupililo cao casweka ngati ngalawa ” cifukwa cosasankha bwino nchito ? M’malo mwake , iye anali kucenjeza odzozedwa kuti sayenela kukhala ngati kapolo woipa . Palibe munthu amene angalankhulile Mulungu ndi kuyankha mafunso amenewo ngati Mulungu sanatifotokozele za iye mwini . ( 1 Pet . 2 : 23 ) Yesu anali kudziŵa kuti kubwezela n’kwa Yehova . ( Aroma 12 : 19 ) Ifenso Akhiristu tikulangizidwa kukhala odzicepetsa ndi kupewa ‘ kubwezela coipa pa coipa . ’ — 1 Pet . NKHANI YA PACIKUTO | ANGELO KODI ALIKO ZOONA ? Kapena pali zina zake zimene zikudetsani nkhawa ? Timafunitsitsa kudziŵa mmene umoyo wathu kapena wa okondedwa athu udzakhalila . ( Ŵelengani Salimo 10 : 4 . ) Kodi adzasangalala ndi zilizonse zimene ndingasankhe malinga ngati siziphwanya malamulo a m’Baibulo ? Kumbukilaninso zimene zinathandiza Abulahamu , Yosefe , na Davide kuyembekezela moleza mtima kukwanilitsidwa kwa malonjezo a Yehova . Kapena bwanji ngati wayamba nchito imene simupatsa nthawi yolalikila ndi kupezeka pa misonkhano ya mpingo ? Akapanga zosankha mwanzelu , amapindula . ( Aef . 2 : 19 ) Ngati tiyesetsa kuona anthu mopanda tsankho , ndiye kuti tikuvala umunthu watsopano . — Akol . Anadalilanso Yehova kuti amutsogolele . ( Deut . Mothandizidwa ndi mzimu woyela wa Mulungu , M’bale Knorr , anaona kuti ofalitsa afunika kuphunzitsidwa mmene angalalikilile . Kuyambila mu 2000 , tapambana milandu 268 m’makhoti akuluakulu padziko lonse . Potengela citsanzo cimeneco , oyang’anila madela akhala akuika akulu na atumiki othandiza paudindo kuyambila pa September 1 , 2014 . Motelo , bungwe lolamulila ku Yerusalemu linatumiza mtumwi Petulo ndi Yohane kwa Asamariya otembenukila kuciyuda . Musafulumile kuganiza kuti iye akucita cinthu cina coipa kwambili mwakabisila . M’bale Russell anakamba kuti “ anthu anali kumvetsela mwachelu ” pamene anali kukamba nkhani yofotokoza za cikhulupililo ca Abulahamu na madalitso amene anthu adzalandila m’tsogolo . Komabe , n’ciani cingacitike mwanayo akadzakula ? Izi n’zimene anatilonjeza Mlengi wathu wacikondi , Yehova Mulungu . Cikhulupililo ca Petulo cinam’cititsa kucita cinthu cimene cinaoneka ngati cosatheka 51 : 10 , 12 ) Conco , ngati tikali kulimbana ndi zilakolako zoipa , Yehova angatithandize kukhala ndi mtima wofunitsitsa kumvela malamulo ake ndi kucita zinthu zoyenela . Atate wathu wakumwamba amamvetsela atumiki ake akamamuuza maganizo ao ndi zakukhosi kwao . Pamene Blossom Brandt anapanga cosankha cakuti abatizike , makolo ake acikhristu anafuna kutsimikizila kuti anali wokonzekadi kutenga sitepi yofunika kwambili imeneyi . Koma pambuyo pake , covala cimeneco cinamubweletsela mavuto . 3 : 1 , 2 , 6 ) Kodi muganiza kuti Timoteyo anamva bwanji atapatsidwa udindo umenewo ? Nanga Yesu anawathandiza bwanji kumvetsetsa mfundo imeneyi ? Kuyambila mu 1919 , Yesu Khiristu wakhala akugwilitsila nchito kapolo ameneyo kuthandiza otsatila ake kumvetsetsa Buku la Mulungu na kutsatila malangizo ake . Kodi vuto linali ciani ? Conco , Ophunzila Baibo ambili analemba makalata olaila machechi awo . Cifukwa ca mphamvu ya kacipangizo ka IUD , dzilalo likaloŵa m’cibalilo silikwanitsa kukhala bwino - bwino kapena kukula cakuti mimba imangopitilila . Timakhala ndi maganizo amenewa kwa nthaŵi yaitali . * — Genesis caputala 37 ndi 39 . Poganizila zimenezi , tinaona kuti ndi bwino kuti pasakhale anthu otilandila , komanso kuti tipewe kukambilana ndi Mboni za kumeneko . Tikakhala mu ulaliki , kodi sitingauzeko ena za amene Anacititsa kuti pakhale dongosolo limeneli ? — Chiv . Kukonda Mulungu mokwanila kudzatithandiza kucita ciani ? Ngati munatsiliza kuphunzila bukuli , bwanji osayamba kuphunzila mabuku ena amene angakuthandizeni kukhala wokhazikika m’cikhulupililo ? ( Akol . Sindifuna kuoneka wadothi ngakhale kuti ndine wacikulile , ndipo ndimapewa maganizo akuti , ‘ zilibe kanthu ndi mmene ndimaonekela . ’ ” Tiyeni tiyesetse kukhala amtendele , ndipo tidzamva monga mmene wamasalimo anamvela pamene ananena kuti : “ Taonani ! Alongo ambili ali ndi luso lophunzila msanga zinenelo zina ndipo amalalikila m’zinenelo zimenezo . Ena amacita bwino kwambili pankhani yolimbikitsa ena ndi kusamalila odwala . Pambuyo pake , ayenela kupanga cosankha cimene cidzawalola kukhala na cikumbumtima coyela pa maso pa Mulungu . Mulungu anayankha kuti : “ Mpaka mizinda yao itaonongedwa n’kukhala bwinja , yopanda wokhalamo . Ndiyeno , ananditulutsa , koma atazindikila kuti ndikali ndi maganizo ofuna kucoka , ananditsekelanso m’cipinda . Masiku ano , mwamunayo amam’limbikitsa kupita kumisonkhano ndipo amam’pelekeza . Ndipo tikumva mmene mtumwi Yohane anamvelela pamene anati : “ Taganizilani za cikondi cacikulu cimene Atate watisonyeza . ” — 1 Yohane 3 : 1 . 17 : 17 ; 25 : 25 . Si anthu onse ali nalo . Mau otsiliza amene Peter analemba , anali opita kwa abululu ake . Baibo imakambanso momveka bwino ponena za colinga ca Mulungu cokhudza anthu . N’zosakaikitsa kuti anawo sanaiŵale zimene anaphunzilapo . BAIBO SI BUKU LA SAYANSI , KOMA PALI ZINTHU ZOONA ZIMENE INAKAMBILATU KALE - KALE ANTHU AKALIBE KUZITULUKILA . ( b ) kukoma mtima kwakukulu ? Masiku ano , gulu la Mulungu padziko lapansi likupita patsogolo cifukwa lili ndi anthu oyanjidwa ndi Mulungu . idzakhala nkhondo ya zida za nyukiliya , kapena kusintha kwa nyengo kowononga cilengedwe . Ndinadabwa kwambili kuona kuti panali zambili zimene sindinazimvetse . Litanthauza kuti pa mavuto alionse amene tingakumane nao , Yehova adzatipatsa mphamvu zofunikila kuti tikwanitse kupilila . ( 1 Pet . N’ciani cimene tikuphunzila pa citsanzo ca dalaivala amene amanyalanyaza kusamalila injini ya galimoto yake ? Nanga zimenezi zikugwilizana bwanji ndi nchito yophunzitsa ena mumpingo ? N’cifukwa ciani Yesu sanali kulimbikitsa Ayuda kudana ndi anthu ena ? Pambuyo pake , tinapemphedwa kupita ku Belize kukaphunzitsa anthu Baibulo . Poona mfundo za m’Baibulo zothandiza , anthu afika povomeleza kuti n’zoona inauzilidwadi na Mulungu . 4 : 8 ) Ganizilani za akulu mumpingo , oyang’anila madela , a m’Komiti ya Nthambi , ndi a m’Bungwe Lolamulila . Anthu amaganiza kuti kucita zimenezi kumawapatsa mwai wocotsa paudindo olamulila osakhulupilika . Ngati makolo ali na cikondi codzimana , mwana aliyense m’banja amapindula kwambili . Kucita zimenezi kumafuna kudzipenda nthawi zonse . Ena angafunike kupanga masinthidwe aakulu paumoyo wao kuti akhale oyela . Iwo amadziona kuti alibe ciyembekezo ciliconse . Cimene cinakhala cofunika kwa ine ni kusangalala na kufuna akazi ambili panthawi imodzi . N’nali munthu woipa mtima , wopondeleza ena ndi waciwawa . Kodi anthu othaŵa kwawo amapindula bwanji tikawalalikila ? Ofalitsidwa na Mboni za Yehova . Cifukwa cakuti ili na mau osavuta kumva , Mau a Mulungu amatifika pamtima . ( Sal . Dzikolo linali la Cikomyunizimu . Anthu ambili m’tauni ya Saxony analibe cidwi na zacipembedzo . Akhiristu apabanja afunika kuyesetsa kuthetsa vuto lililonse tsiku lisanathe . Patapita zaka , nthawi ina Petulo analeka kudya cakudya na Akhristu a ku Antiokeya amene sanali Ayuda . ( Agal . Paulo atamva izi , anadziŵa kuti n’zimene Yehova anali kufuna , ndipo mosazengeleza anavomela ciitanoci . Iye anali ndi mtima wodzipeleka . Kodi anthu ena angapindule bwanji ngati titumikila Mulungu modzipeleka ? Zimenezo zinali kuphimba kwambili mfundo zothandiza zofunika kuphunzilapo pa nkhanizo . ( Machitidwe 2 : 42 ) Mwacionekele , inunso mumayembekezela mwacidwi tsiku la misonkhano kuti mukasonkhane . Imeneyo ndiyo inakhala nyumba yathu . Nanga bwanji ngati mwadziŵa kuti muli ndi maganizo olakwika ponena za anthu a m’dziko lina , a cikhalidwe ndi cinenelo cina kapena a fuko lina ? Mau a Mulungu anathandiza wolemba Salimo 119 kukhala wosiyana ndi ena . Kodi imwe munalaŵako ubwino wa Yehova ? Akhristu amene makolo asankha kuti athandize ana awo mwauzimu , afunika kukamba zinthu zimene zingalimbikitse anawo kulemekeza makolo awo . ( Yoh . 2 : 18 - 21 ) Mwina , Yesu anaona kuti n’kosafunika kuyankha Asadukiwo acinyengo , amene sanali kukhulupilila ciukililo kapena kukhalapo kwa angelo . ( Miy . 23 : 9 ; Mat . Ulosi wa pa Danieli capitala 4 unalembedwa kuti anthu adziŵe kuti “ Wam’mwambamwamba ndiye Wolamulila wa maufumu a anthu . ” Moleza mtima muthandizeni kuganizilapo pa nkhaniyo . Ananiphunzitsa kuseŵenzetsa galamafoni kuti tizilizila anthu nkhani zazifupi za m’Baibo zojambulidwa . Iye anaganizila lemba la Miyambo 20 : 11 imene imati : “ Ngakhale mnyamata amadziwika ndi nchito zake , ngati zocita zake zili zoyela ndiponso zowongoka . ” Malemba amati , “ Yehova anadalitsa kwambili mapeto a Yobu kuposa ciyambi cake , ” ndipo pambuyo pake “ anakhalanso ndi ana aamuna 7 ndi ana aakazi atatu . ” Nkhondo yoyamba ya padziko lonse inali yaikulu cifukwa cakuti inapha ndi kuvalaza anthu ambili . Ndinaona kuti umenewu unali ubale wa padziko lonse . Baibo imati : “ Nzelu imatsimikizilika kuti ndi yolungama cifukwa ca nchito zake . ” Pa Aroma 15 : 4 , mtumwi Paulo anati : “ Zinthu zonse zimene zinalembedwa kalekale zinalembedwa kuti zitilangize , zimatipatsa ciyembekezo cifukwa malembawa amatithandiza kupilila ndiponso amatilimbikitsa . ” Touma ) , — September - October Mu 1937 , ang’ono awo a amayi ndi amuna awo amene anali a Mboni , anabwela kudzaticezela kucokela ku France ndipo anatisiyila mabuku ochedwa Government ndi Deliverance , ofalitsidwa ndi Watch Tower Society . Akangoyang’ana pa kacizindikilo kenakake , kompyutayo imatumiza uthenga umene umasinthidwa kukhala mau . ( Akol . 4 : 10 ) Ganizilani mmene Baranaba anamvelela pamene Paulo anapempha Maliko kuti azim’thandiza . — 2 Tim . N’kusiyana kwabwanji kumene kunalipo pakati pa atsogoleli a anthu a Mulungu ndi a mitundu ina ? Yehova wakhala akunithandiza mogwilizana ndi lonjezo lake lakuti adzathandiza ana amasiye . Ndinadzifunsa kuti , ‘ Nanga iye ali kuti ? ( Oweruza 13 : 9 ) Makolo , nanunso Yehova adzamvetsela mapemphelo anu . Macaputala ndi mavesi amakuthandizani kupeza nkhani imene mufuna m’Baibulo . Ise tinali kumva zonsezi tili m’cipinda cathu capamwamba . N’ciani cimene tiyenela kucita kuti tikhale olimba kuuzimu ndi kukhalabe ndi moyo ? Pokambilana ndi mai wacisamariya , Yesu anakambanso kuti “ nthawi ” “ idzafika ” imene kulambila Mulungu mwa njila imeneyo kudzasintha . Yehova amafuna kuti tizikamba naye . Iwo amacita zinthu mwacikati - kati ndipo amapeza cimwemwe ponse paŵili , pogwila nchito komanso panthawi yopumula . Onani zimene ena mwa iwo anakamba : 1 : 5 - 8 , 14 - 17 . Ndi mmenenso zilili masiku ano . Kucita zimenezi kumapangitsa kuti Yehova alemekezeke . — Eks . Raquel anati : “ Pamene mwamuna wanga ananisiya , cinaniŵaŵa kwambili , ndipo n’nakhumudwa . ( b ) Kodi onse amene amadziŵika ndi dzina la Mulungu ali ndi udindo wotani ? Cocitika cimeneco cionetsa phindu lofunsa mafunso oyenelela mwaluso . Mwina muli na matenda aakulu ndipo muona kuti palibe cizindikilo cakuti mucila . mu umoyo wanu ? Ndiye cifukwa cake Yehova amafuna kuti tikhale odzipeleka kwa iye yekha . Mose ni mmodzi mwa anthu amene anadalitsidwa mwanjila imeneyi . Timasemphana maganizo na Akhristu anzathu cifukwa tonse ndise opanda ungwilo . Aliyense wa ise angakwanitse kukhala na umunthu watsopano . Nthawi zonse ndinali kupemphela kwa Yehova . Kodi kugwilizana kwa zipembedzo kungathetse mavuto pakati pao ? YANKHO : Yesu ni Mwana woyamba kubadwa wa Mulungu . Anthu kumeneko anali kumvetsela uthenga wa Ufumu . Nanga bwanji zolinga zake zokhudza maphunzilo na nchito ? Kodi Mau a Mulungu amatithandiza bwanji kucita zimenezi ? ( Numeri 15 : 38 - 40 ; Mateyu 23 : 5 - 7 ) Koma mosiyana na iwo , Yesu analangiza atumwi ake kuti ‘ asamacite ulamulilo pa ’ ena . Yehova anapanga anthu a mitundu yosiyanasiyana , ndipo zimenezi n’zabwino ndiponso zokondweletsa . Koma dziko loipali linaŵeluzidwa kale kuti lidzawonongedwa . ALLEN * anati : “ N’nali kumvela mantha kukukila kuno . Pakati pa Ayuda otengedwa ukapolo panali atumiki a Mulungu okhulupilika . Iwo anavutitsidwa pamodzi na mtundu wocimwawo . Ndiponso , atumiki anzanga a ku maiko ena anithandiza kukhala woganiza bwino . Kodi Mfumu Hezekiya anacita ciani ? Timamutamanda , kumuyamikila , ndi kumupempha kuti atitsogolele . Ndipo ayenelanso kukonda mnzake mmene amadzikondela yekha . Kudzela mwa Abulahamu , Mulungu adzautsa mbeu imene idzabweletsa madalitso kwa anthu onse . Mwacionekele , Yehova anafuna kuti pakhale atumwi 12 kuti akakhale “ miyala yomangila maziko yokwana 12 ” a Yerusalemu Watsopano . ( Luka 13 : 10 - 13 ) Mwa cikhalidwe cawo , Yesu anaseŵenzetsanso mau amenewa ngakhale kwa amayi ake . Pa nthawiyo , m’bale Bright anayamba kuphunzila Baibo na mkulu wa apolisi . 24 : 10 ) Mau a Mulungu amaonetsa kuti kukhala “ kapolo wa cilamulo ca Mulungu ” ndiye cinthu canzelu . 30 : 11 - 14 . Mulungu amafunanso kuti tizilemekeza ufulu wa ena pa zosankha zawo . Kudzoza munthu kukhala mtsogoleli wa anthu ndi kosiyana kwambili ndi kuphunzitsa m’bale kuti ayenelele kukhala mkulu kapena mtumiki wothandiza mumpingo . Mkristu wofikapo amatsatila ‘ mapazi a Yesu mosamala kwambili . ’ Dzifunseni kuti , ‘ Kodi cinthu coyamba cimene nifunika kucita kuti nikwanilitse colinga canga n’ciani ? ’ Nyumba za Ufumu zambili zatsopano zifunika kumagidwa . “ Ife timasonyeza cikondi , cifukwa iye ndi amene anayamba kutikonda . ” — 1 YOHANE 4 : 19 Ndiyeno a Doris anauza Katherine kuti : “ Yehova amakugwilitsila nchito kundithandiza . mungathetsele mavuto akabuka . Mfumu Davide anali ‘ kufunitsitsa ndi mtima wake wonse ’ kumanga nyumba ya dzina la Yehova . N’zinthu ziti zimene zingalengetse munthu kukhala wodetsedwa pamaso pa Mulungu ? ( Gen . 14 : 22 , 23 ) Yesu anagogomeza kufunika kwa cikhulupililo cotelo , pamene anauza mnyamata wina wacuma kuti : “ Ngati ukufuna kukhala wangwilo , pita kagulitse katundu wako ndipo ndalama zake upatse osauka . Cinapeleka malangizo akuti zimenezi zikacitika , munthu anali kufunika kuyeletsedwa na madzi , motsatila mwambo wa m’cilamulo . Mwakutelo , akulu amaphunzitsa abalewo kukhala na makhalidwe ofunika kwa akulu monga cikhulupililo , kuleza mtima , na cikondi . Kodi kuseŵenzela pamodzi ndi acicepele kungakhale kothandiza motani ? Kukonda Yehova kwandithandiza kuti ndisamangoganizila zinthu zoipa zimene ndinaona kunkhondo ndiponso kwandithandiza kupilila mavuto ena Oyendetsa ngalawa akale anali kudziŵa bwino kuti kuyenda panyanja ya Mediterranean m’nyengo yamphepo kunali koopsa . Paulo anali citsanzo cabwino pankhani yolemekeza ufulu wa abale ake wodzipangila zosankha . Kugwilitsila nchito mankhwala otelo n’koopsa . Ndi vuto lotani limene limakhalapo ngati munthu nthawi zonse amangodandaula za amene akutsogolela ? Cisumbu ca mwala cochedwa Makrónisos , cili pafupi na cigawo ca Attica , pamtunda wa makilomita 50 kucokela mumzinda wa Athens . Ndikhulupilila kuti mudzasangalala kwambili ndi nkhani zili m’magaziniwa . Pambuyo polenga kumwamba ndi dziko lapansi , Yehova anapanga zolengedwa zina zimene zinadzakhala mbali ya banja lake . M’kupita kwa nthawi , mu ulamulilo wa Mfumu Theodosius Woyamba ( 379 mpaka 395 C.E . ) , Chechi ya Akatolika ( Cikhiristu codetsedwa ) , inakhala cipembedzo covomelezedwa ndi Ufumu wa Roma . Salimo 40 : 17 ; Yehova ndi dzina la Mulungu monga mmene Baibulo limanenela . Komabe , kucita izi sikungakhale kothandiza kweni - kweni . Kenako , tiyenela kutsatila mapazi ake . Ngakhale kuti cilangoci cimaŵaŵa , pambuyo pake cimakhala ndi zotsatila zabwino . Ndithudi , zosangulutsa n’zofunika pa umoyo wa munthu . Pakuti cifukwa ca iye tili ndi moyo , timayenda ndipo tilipo . ” — Machitidwe 17 : 25 , 28 . Komabe , pali nsembe zinanso zimene Mulungu amakondwela nazo . ( 1 Mafumu 17 : 1 ) Izi zinatheka cifukwa ca dzanja la Mulungu , koma Ahabu analephela kukhulupilila zimenezi . ( Maliko 6 : 31 , 32 ; Yohane 2 : 2 ; 21 : 12 , 13 ) Yesu sanali cabe mphunzitsi wao , koma analinso mnzao wapamtima . Cihema ca Mulungu cili pakati pa anthu . Iye adzakhala pamodzi nao , ndipo io adzakhala anthu ake . M’nkhani yotsatila tidzayankha funso limeneli . Nthawi zina , tingakhale na nkhawa kwambili cifukwa ca mavuto amene takumana nawo . 1 : 28 ) Nowa anapatsidwa malangizo osapita m’mbali opangila cingalawa kuti anthu akapulumukilemo pa Cigumula . Ngati muŵelenga Baibo , mudzapindula na malangizo ocokela kwa Mulungu , ndiponso mudzamudziŵa monga mnzanu . Mu 1934 , gulu la Yehova linayamba kupanga magalamafoni onyamulila m’manja opita nao mu ulaliki . Anthu akhoza kupewa mavuto onsewa ngati atsatila malangizo anzelu a m’Baibo . Paulo anakakamizika kucoka kumeneko , koma anali ndi cikhulupililo cakuti Timoteyo adzapita kukalimbikitsa abale kumeneko . ( Mac . 17 : 5 - 15 ; 1 Ates . Komanso , n’kutheka kuti tinapita patsogolo mwauzimu , koma pambuyo podzipendanso bwino , tingaone zinthu zina zimene tifunika kucita kuti tikhale ofikapo mwauzimu . Nanga cifukwa ciani ? Cinthu cina cofunika cimene cingathandize cikwati kukhala colimba ndi kulankhulana mokoma mtima . Pamene tiphunzila zambili za Yehova , cikumbumtima cathu cidzatithandiza kuzindikila mwamsanga zimene iye amaona kuti n’zabwino kapena zoipa . Kuwonjezela pa kulimbitsa cikhulupililo cathu , kukambilana mmene Baibo yatetezekela m’zaka zonsezi , kumalimbitsa cikondi cathu pa Yehova . Pali zifukwa zambili zimene Mulungu amatiuzila kuti tisamatenge mbali m’ndale . Iye anali kudziŵa bwino zoyenela kukamba cifukwa cakuti Yehova anamuphunzitsa ‘ mmene angayankhile munthu wotopa . ’ “ MPAKA liti ? ” ( Machitidwe 17 : 26 ) “ Mulungu alibe tsankho . Iye amalandila munthu wocokela mu mtundu uliwonse , amene amamuopa ndi kucita cilungamo . ” — Machitidwe 10 : 34 , 35 . Kukwanilitsidwa kwa ulosi wa conco kukanacititsa kuti woloselayo adziŵike . Cifukwa ca kuculuka kwa nthawi imene amathela mu ulaliki ndi kuthandiza m’njila zina , io alibe nthawi yambili yakuti aseŵenze . N’cifukwa ciani acikulile afunika kuthandiza acinyamata kutenga maudindo aakulu ? Nditaŵelengela mtengo ndinaona kuti zingakhale bwino kugulitsa nyumba kuti tilipile loni , ndiyeno ndalama zotsala zingatithandize pa zosoŵa zathu kufikila nditatenga penshoni . Mfumu Sauli anamva za mbili yake . Cifukwa ca cifundo , Yesu anacita zinthu zimene anthu sanali kuyembekezela . Ndipo kambilanani nkhaniyo ndi akulu mu mpingo , woyang’anila dela , kapena amene anatumikilako ku maiko osoŵa . Nimawayewa ngako amuna anga , koma kucita upainiya kumanithandiza kupilila . APRIL 7 - 13 , 2014 | TSAMBA 8 • NYIMBO : 99 , 107 Anapitilizabe kuucitila cifundo , ndipo anakhalabe wokhulupilika pa pangano lake ndi iwo . 24 : 10 ; Afil . ( 3 ) Kodi aliyense payekha angalimbikitse bwanji mgwilizano ? Alongo amenewa ndinawalemekeza cifukwa anali a zaka zofanana ndi amai . John Wischuk Ndinamuuza nkhani zosangalatsa zili m’magazini amene munandipatsa . Umafunikilanso kuphunzila zikhalidwe ndi zinthu zatsopano . ” Nkhope ya Ahabu inasintha cifukwa ca ukali ndi cidani , ndipo mwaukali anati : “ Wandipeza kodi mdani wanga ? ” — 1 Mafumu 21 : 20 . M’kupita kwa nthawi , zinakhalanso zosavuta kupanga mapepala ndi kukonza mabuku . Tikambilananso mmene odzozedwa ayenela kudzionela ndi mmene ife tiyenela kumvela tikaona kuti ciŵelengelo ca anthu amene amadya mkate ndi kumwa vinyo pa Cikumbutso cikukwela . Ku sukulu ya sekondale mumzinda wa Glenorchy pa cilumba ca Tasmania , ndinapatsidwa mphoto zambili cifukwa cocita bwino m’maphunzilo . N’cifukwa ciani Akristu amayamikila kukhala ndi okalamba mumpingo ? Mfundo za m’Baibulo zimene takambilana sizigwila cabe nchito pankhani yokhudza zosangulutsa . SIKUDZAKHALANSO NKHONDO Ngakhale kuti kudziŵa ziphunzitso zoyambilila n’kofunika , tifunikila kudya “ cakudya cotafuna , ” cimene ndi ziphunzitso zozama za m’Baibulo . Cimene cinali kuoneka ngati ndodo wamba cinasanduka njoka cifukwa ca mphamvu ya Mulungu . Nkhani ziŵilizi zitithandiza kupenda mafanizo 7 amene Yesu anakamba . Kaya tiŵelenga Mau a Mulungu m’Baibo mweni - mweni , pa foni , kapena pa tabuleti , colinga cathu ciyenela kukhala cakuti tiwamvetsetse ndi kuwalola kusintha umoyo wathu . Mu 1943 , anaphedwa pa nkhondo ku Russia . Nthawi zina , mungafune kucita cinacake , koma pambuyo poganizilapo bwino , mungasinthe maganizo anu . Koma zimene zinacitika mwina zinali zosiyana na zimene Mariya anali kuyembekezela . 2 : 12 ) Koma “ mwacikondi ” cake , Yehova anatikokela kwa iye . Cinthu cacitatu cimene cingatithandize kupewa zandale , ndi kudalila Yehova . ( Machitidwe 1 : 8 ; 1 Petulo 4 : 14 ) Anthu ena acipembedzo amakamba kuti “ Tili ndi mzimu woyela . ” Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lafalitsidwa m’zitundu zambili . Tikacitita zimenezi , Yehova adzatiyanja ndi kutidalitsa , monga mmene anacitila ndi Yosefe . Yesu anali kudziŵa dzina la Mulungu ndipo analiseŵenzetsa . — Yohane 17 : 25 , 26 . 5 : 41 ) Inunso mukakumana ndi cizunzo muyenele kutengelapo mwai wotsatila citsanzo ca Petulo , ndi kutsatila mapazi a Yesu mwa kuonetsa mzimu wodzimana . 40 : 5 - 13 . “ N’CIFUKWA ciani zimenezi zandicitikila ? ( Yoh . 3 : 16 ) Paulo anakamba kuti Yesu ‘ anamuveka ulemelelo ndi ulemu ngati cisoti cacifumu cifukwa cakuti anazunzika mpaka imfa . Ida na Filip ( Luka 18 : 1 ) Tiyenela kupitiliza kupempha Mulungu kuti azititsogolela ndi kutithandiza , tikatelo tidzakhala ndi cikhulupililo . Zimene timaganiza zimakhudzanso thupi lathu . Muzikhulupililanso kuti cifukwa ca dipoli , inu muli na ciyembekezo ca moyo wosatha . 1 : 14 . Koma zaka 10 zapitazo , iye sanali kukonda kulalikila . Phunzilani ku Mbalame , Na . Koma cimene cimandithandiza ndikayamba kuganiza zimenezo , ndi kuthandiza munthu winawake kugwila nchito iliyonse . ” Mphatso ya mtendele . Herode anakondwela ndi citamando cimeneco . Amuna amenewa anayamikila kwambili utumiki umene Mulungu anawapatsa . Yehova ndi Mpatsi Wamkulu cifukwa cakuti amatipatsa zinthu zambili . Njila zimene olosela amaseŵenzetsa pofuna kudziŵa zakutsogolo zimasiyana - siyana , koma zimene amapeza kambili sizigwilizana . 11 : 1 . N’cifukwa ciani kuvomeleza za Mulungu kaya za cisanduliko , konse kumaloŵetsapo cikhulupililo ? Koma Yehova watidalitsa pa nchito yolalikila . Izi zinamufooketsa kwambili Rhonda koma pamene anayamba kupezako bwino anayamba kucita upainiya wa nthawi zonse . Nanga anaonetsa bwanji makhalidwe amenewa ? Citsanzo ca Mfumu Sauli cionetsa mmene kudzikonda kungaonongele mzimu wodzimana . Kukhala ndi moyo m’dziko latsopano sikutanthauza kuti tidzakhala ndi ciliconse cimene tafuna panthawiyo . Mulungu “ amakonda cilungamo . ” N’zoonekelatu kuti tifunika kugwilitsila nchito cikumbumtima cathu cophunzitsidwa bwino posankha zosangulutsa . M’nthawi ya atumwi , Mulungu anakana mtundu wosakhulupilika wa Aisiraeli . William anati : “ Kuphunzila cinenelo , kucita upainiya , kusamalila mpingo , ndi kupeza ndalama zokwanila kusamalila banja , nthawi zina kumakhala kolemetsa . ” Zimenezi zili ngati coonadi “ cakale ” m’lingalilo lakuti tinazidziŵa ndi kuzimvetsetsa titangokhala Mkhristu . N’cifukwa ciani mbeu ya mkazi inafunikila kutetezedwa ? Kodi mumayamba kuganiza kuti munasankha mwamuna kapena mkazi wosayenelela ? kusintha m’zandale ? Wosimba ni Pavel Sivulsky Onse amenewa , poyamba sakhala omasuka , amacita cilendo . N’nadziŵa kuti Yehova adzathetsa kupanda cilungamo m’njila yoyenela ndiponso panthawi yoyenela . KULIMBIKITSA MGWILIZANO WENI - WENI Makina opimila zinthu za mlenga - lenga ochedwa Space Station anapangidwa ndi anthu ocokela m’maiko 15 . Kucita zimenezi kudzakupatsani mwai woona maluso ao , kuwayamikila , ndipo io adzapita patsogolo . — Miy . 5 : 42 ; 20 : 20 ) Malinga ni mmene zinthu zilili pa umoyo wathu , tingacite bwino kuona njila za mmene tingawonjezele utumiki wathu . Khamu la anthu linadabwa kuona cuma cambili cimene cinali kudutsa m’miseu ya mu mzinda wa Roma . Conco , kuti nikhale pa ubwenzi na anthu amene amakonda Mulungu , n’nakonza ndandanda ya zocita zauzimu zimene ningacitile nawo pamodzi . Ngozi zoopsa kwambili ndi matenda aakulu amakhudza munthu wina aliyense mosasamala za msinkhu kapena umoyo wake . Mlongo wina wa ku Kenya , dzina lake Sarah , anati : “ Ndinapemphelela wophunzila Baibulo amene ndinaona kuti sayamikila zimene anali kuphunzila . Nanga n’cifukwa ciani ? Pokambitsilana , makolo muyenela kudziŵitsa banja lanu zimene mufuna , kuculuka kwa ndalama zimene mufunikila ndi zinthu zina . Wolemba mbili yakale Josephus anakamba kuti malowa anali pamwamba kwambili cakuti ngati munthu waimililapo n’kuyang’ana pansi , “ anali kucita cizwezwe . ” 18 Kodi ‘ Mumasunga Nzelu Zopindulitsa ’ ? Tsopano ndifuna kukufotokozelani za cikondi canga ca poyamba kwa Yehova . ( Chiv . Kodi mumamva bwanji mukaona mmene Yehova adzayankhila pempho lathu lakuti cifunilo cake cicitike pa dziko lapansi ? Masiku ano , olambila oona a Yehova amayesetsa kukhala odzicepetsa ndi omvela . Mwacitsanzo , cifukwa ca cikhulupililo timakwanitsa kulimbana ndi Mdyelekezi , mdani wathu wamphamvu . Posayamba wafunsila kwa mwamuna wake , iye ananyozela umutu wa Adamu . Koma cokondweletsa n’cakuti abale amaika mtima wawo wonse pa nchito yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu . N’cifukwa ciani tifunika kupewa mkwiyo ? Conco , inu akulu okondedwa , pophunzitsa ena muziyesetsa kukhala bwenzi la wophunzila osati cabe mphunzitsi . — Miy . Atate anali munthu wocepa thupi , koma wathanzi ndi wamphamvu . Iwo anali kukonda kugwila nchito zovuta . Ndipo ise tonse anatiphunzitsa kukonda nchito . 4 : 11 ) Rune , mpainiya amene watumikila kwa zaka 16 , anati : “ Nimayamikila ngako mwayi umene nili nawo wocitila umboni za Mlengi wa cilengedwe conse . Muzicita zimenezi poyembekezela ndi kukumbukila nthawi zonse kukhalapo kwa tsiku la Yehova . . . Mungacite zimenezi m’njila zosiyana - siyana . Ameneyutu adzachedwa Mkazi . ” — Gen . Kodi banja lalikulu lingadye masiku angati cakudya cimeneco ? Ni ciyembekezo canji cimene amuna ndi akazi akale acikhulupililo anali naco ? Iwo anali kukambilana mmene Yehova anawathandizila kuti afike pamsonkhanowo . Nanga ni mapindu abwanji amene mungapeze ngati mwakhala na cikhulupililo colimba pa zimene muyembekezela ? Umoyo wanga ni wodzala na cimwemwe ndi madalitso osaneneka . ” Koma nthawi zambili , tinali kungogwila nchito . Anthu 15 mwa anthu amene Irene anaphunzila nawo Baibo , anabatizika . Kwa mlungu wonse n’nacezela kufufuza mayankho a mafunso amene ananifunsa . Komabe , ali ndi zaka 40 , Mose anapanga cosankha cimene cinadabwitsa banja lacifumu laciiguputo limene linali kum’sunga . Stephen wa ku Australia , amene ni kholo anakamba kuti : “ N’nali kukonda kukamba mau onyoza ndiponso n’nali kukwiya kaŵili - kaŵili pa nkhani zing’ono - zing’ono . ( 1 Akor . 10 : 13 ) Izi sizitanthauza kuti tizingokhala cabe , n’kumayembekezela Yehova kuti atithetsele mavuto . 38 : 6 , 15 . Onani Nsanja ya Olonda ya October 15 , 2013 , mapeji 17 - 20 . Ndipo kuusunga kumaphatikizapo kuphunzila kukonda dzina la Mulungu ndi kulilemekeza kwambili . — Sal . Ena amamvetsela , koma ena amadana nao . 7 : 2 , 3 . ( Machitidwe 5 : 29 ) Koma nthawi zonse tikasankha kumvela Yehova , iye amakondwela . — Miyambo 27 : 11 . 5 : 16 . Tingakaikilenso kuti ndife oyenelela kudzalandila mphoto iliyonse . * Kodi timabala bwanji mbewu zatsopano za Ufumu ? Komabe , Mulungu sanakondwele na kulambila kwake , cifukwa maganizo oipa anayamba kuzika mizu mu mtima mwake . Mlongo wina wa ku France anafotokoza vuto limene anali nalo . Iye anati : “ Yehova waniphunzitsa kukhala munthu wacikondi , kugaŵana zinthu ndi ena , na kukonda anthu a mitundu yonse . Apanso , Yefita anatsatila mfundo za m’Cilamulo ca Mulungu kuti asankhe mwanzelu . William Turner , Jr . Mwacitsanzo , taganizilani za fanizo la Yesu la anamwali 10 . Kale , zofalitsa zathu zinali kufotokoza kuti nyali , mafuta , ndi mabotolo a mafuta amaimila zinthu zinazake kapena winawake . Iye anam’tsimikizila kuti mlongoyo sanacitile dala pofuna kum’khumudwitsa . Onani mbili ya Ophunzila Baibulo m’dziko la Britain panthawi ya nkhondo yoyamba ya pa dziko lonse m’nkhani yakuti “ Kale Lathu — Anakhalabe Okhulupirika pa ‘ Ola la Kuyesedwa . ’ ” Nkhaniyi ipezeka mu Nsanja ya Olonda ya May 15 , 2013 . Anali osiyananso ndi anthu okonda umoyo wawofu - wofu , amene anali ‘ kukhala pansalu zokwela mtengo . ’ Ufumu wa Mesiya ndiwo njila yokha imene Yehova adzagwilitsila nchito kuti akwanilitse cifunilo cake ca dziko lapansi ndi ca anthu . Izi zinalimbikitsa abale kupitiliza kugwila nchito yolalikila . 3 : 14 , 15 ) Pamenepa , Paulo anachula zinthu zitatu , ( 1 ) kudziŵa malemba oyela , ( 2 ) kukhulupilila pambuyo pokhutila na zimene anaphunzila , ndi ( 3 ) kupeza nzelu zomuthandiza kuti akapulumuke kudzela m’cikhulupililo cokhudza Khristu Yesu . Zoonadi , unali mwayi waukulu kutumikila pamodzi na amuna okhulupilika ndi auzimu amenewa . — Sal . Yehova anapeleka dipo n’colinga cakuti anthu omvela amasulidwe ku ucimo ndi imfa . Kodi inu mudzadzipeleka ? Taphunzilapo ciani pa zitsanzo zimene tafotokoza m’ndime zapitazi ? Ophunzila Baibulo anali kudziŵa kuti ayenela kulalikila , ndipo anali kucita khama kufotokoza zimene Baibulo limaphunzitsa . Ciwombankhanga cimachulidwa kaŵili - kaŵili m’Baibo ndipo zithunzi zake zinali zojailika m’Dziko Lolonjezedwa . Makolo acikhiristu ali na udindo wophunzitsa ana awo kutsatila mfundo za m’Baibulo . Conco , Mkristu ayenela kukhala ndi cikhulupililo colimba kuti akane kucita zinthu zimene acibale ake afuna koma zimene sizisangalatsa Yehova . Taganizilani citsanzo ca Carin . Tate amakonda ana ake ndipo safuna kuti io azisoceletsedwa ndi kunamizidwa . 51 : 1 , 17 ; 63 : 1 . Mwina ayi . Ngakhale kuti Cathy alibe zinthu zambili , iye ali ndi cimwemwe . Ndiyeno , uthenga wabwino unafalikila kwa Asamariya , ndipo panakhala zotsatilapo zabwino . 14 , 15 . ( a ) Kodi makolo acikristu ayenela kukhala ndi colinga cotani ? Lembali limanena za “ maziko olimba a Mulungu , ” ndiyeno limachulanso za mauthenga aŵili ozokotedwa pamenepo . Uthenga woyamba ndi wakuti “ Yehova amadziŵa anthu ake . ” 8 KODI YESU ANALI KUONEKA BWANJI KWENI - KWENI ? Ziwanda n’zoipa kwambili . Zimatsutsa Yehova ndi kusonkhezela anthu ambili kusamvela malangizo ake . Mu 1919 , “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” anaikidwa kuti azipeleka cakudya cauzimu kwa a pa banja la cikhulupililo . ( Mat . “ Nimayamikila ana anga kaŵili - kaŵili cifukwa cokhala omvela m’dziko limene ambili ni osamvela . 18 , 19 . M’munda wa Edeni , Satana anaonetsa monga kuti anali kufunila Hava zabwino , koma m’ceni - ceni zocita zake zinali zadyela ndi zacinyengo . ( Gen . 1 , 2 . ( a ) Kodi makolo ena amene ali ndi ana acinyamata amada nkhawa ndi ciani ? Ena mwa Akhristuwo anali kucita cigololo cauzimu mwa kukhala paubwenzi na dziko . ( Yak . ( Yoh . 15 : 19 ; 1 Yoh . 8 : 1 ) Yesu anadziŵa kuti otsatila ake ambili adzakakamizika kusiya nyumba zawo . Mulungu wandithandiza kupanga zosankha zabwino , ndipo pano ndili naye pa ubwenzi wabwino . Iwo anadziŵa kuti mnyamatayo anali atafadi , ndipo anaukitsidwa . Komanso , caposacedwapa mkazi wanga anadwala kwambili . Tidzasangalala kuona dzina la Yehova litayeletsedwa ndiponso kuona Ufumu wake ukulamulila cilengedwe conse . ( Mat . Pa msonkhanowo , panagwa cimvula camphamvu cimene cinaipitsa madzi ambili amene tinali kumwa . Pamene Paulo anali kulembela kalata Akristu aciheberi , anadziŵa kuti pakapita zaka zocepa , ena adzasiya nyumba zao ndi katundu wao . Anali atafa ku umoyo wawo wakale . Tinapita kukakhala ku hotela . Adani a Yesu anafuna kum’kola kuti atengeko mbali m’mikangano yokhudzana ndi za misonkho . ( a ) N’ciani cinacitikila Petulo pa Nyanja ya Galileya ? Abale ndi alongonu , dziŵani kuti Yehova amamvetsa mavuto amene mukukumana nao ndipo amayamikila zonse zimene mumacita kuti mum’lambile . ( b ) Kodi atumiki a Mulungu adzacita ciani panthawiyo ? Limbitsani Cikhulupililo Canu pa Zimene Muyembekezela , Oct . Tiyeni tione mmene mungacitile zimenezi . Kodi tingaphunzile ciani m’fanizo la Yesu la mpesa ndi la wofesa mbewu ? Iye ananithandiza kudziŵa zimene niyenela kucita ndi zimene niyenela kupewa , ndipo zimenezi zinanithandiza kucita utumiki wanga mosangalala . ” Ali wosokonezeka maganizo , Yosefe anayesayesa kuona mmene angatulukile koma analephela . N’zoonekelatu kuti Baibulo ndi buku lothandiza kwa munthu aliyense . Komabe , mdani wathu Satana Mdyelekezi amafuna kuononga cikhulupililo cathu . ( Chiv . ( Onani ndime 9 ) Popeza kuti anthu ambili anali kukamba Cigiriki , mabuku a Mateyu , Maliko , Luka , ndi Yohane analembedwa m’Cigiriki . Iye anali kukana kulandila Akhristu apaulendo , ndipo anali kukopanso ena kuti atengele khalidwe lake . ( 3 Yoh . Pamene mapeto akuyandikila , tiyeni tonse tipitilize kutumikila Yehova ndi kutsatila Kristu monga gulu limodzi la nkhosa . Kodi Yehova adzacita ciani ? Njila ina yofunika kwambili imene ingathandize kuti banja likhale lolimba ndiyo kukhululukilana . Iye ananenanso kuti Yezebeli adzaweluzidwa . — 1 Mafumu 21 : 20 - 26 . Kukonda Yehova kumatilimbikitsa kusinkhasinkha za cilengedwe cake ndi nchito zake zodabwitsa . Koma funso ndi lakuti , Kodi inuyo mukumucitila ciani Mulungu ? Anthu ambili - mbili afa ndi kuvutika cifukwa ca njala . Kuyambila kale - kale , anthu akhala akufunsila kwa olosela zakutsogolo . * Mwa kuika Mwana wake monga Mfumu Mesiya , Yehova anakhaladi Mfumu mwa njila ina . Koma Aroma akucitapo kanthu mwamsanga . Tingavutike ndi matenda osacilitsika , tingatsutsidwe ndi acibale kapena kuzunzidwa kwa nthawi yaitali . ( Aroma 12 : 21 ) Mau akuti “ musalole kuti coipa cikugonjetseni , ” aonetsa kuti tingakwanitse kugonjetsa coipa . Nthawi zina , ifenso tingafunike kusintha cosankha cathu ngati zinthu zasintha kapena ngati tadziŵa mfundo zina zimene poyamba sitinali kuzidziŵa . — w17.03 , mapeji 16 - 17 . Akhristu onse ayenela kukhala na colinga cophunzila zambili osati kungodziŵa cabe ciphunzitso “ coyambilila ca Khristu . ” Ngati munthu walema na kutumikila Yehova kapena kutsatila mfundo zacikhristu , safunika kukamba kuti sanadzipeleke zeni - zeni kwa Mulungu , kapena kuti ubatizo wake unali wosayenelela . Motelo n’zosadabwitsa kuti anthu ambili amaganiza kuti andale ndi amene amacita ziphuphu kwambili kuposa anthu onse . Komabe , kusiyana zibadwa kungayambitse mikangano . Mwacitsanzo , Aisiraeli anali kupeleka nsembe za nyama , ndipo Akhristu nthawi zonse akhala akupeleka nsembe zotamanda Mulungu . Yesu anati : “ Odala ndi anthu amene amazindikila zosoŵa zao zauzimu . ” Nanga tifunika kucita ciani akatipatsa cilango ? Nanga n’ciani cingathandize kuti nkhanza itheletu ? N’cifukwa ciani Aisiraeli analephela kupanga cosankha mwanzelu ? Sayankha Rudolf anapilila mayeselo onsewa . Ngakhale kuti anali wokalamba ndi wathanzi lofooka , anali mpainiya komanso mkulu pamene nkhani ya mbili yake inatuluka mu Nsanja ya Olonda ya August 1 , 1997 , masamba 20 - 25 . Koma cimene tidziŵa n’cakuti Timoteyo nthawi zonse anali kucita zimene angathe kuti atonthoze ndi kulimbikitsa Paulo ndi anthu ena . Iye anakamba kuti , kuyamikila ena mocokela pansi pamtima ndi njila imodzi yofunika yophunzitsila ena . 5 : 29 ) Monga kale , masiku ano alongo athu pamodzi ndi alambili onse amacilikiza ulamulilo wa Yehova . ( Yesaya 65 : 21 ) Komanso “ palibe munthu wokhala m’dzikolo amene adzanene kuti : “ Ndikudwala . ’ ” — Yesaya 33 : 24 . Izi zinatheka cifukwa anakhala Akhiristu obatizika , ndipo Mulungu anawakhululukila macimo kupitila mwa dipo , ndi kuwayesa olungama monga ana auzimu . — Aroma 3 : 23 - 26 ; 4 : 25 ; 8 : 30 . Kodi Yesu anali kucita ciani cifukwa comvela cifundo ena ? “ Ana akakhala aang’ono amamasuka kuuza makolo awo zonse za kumtima . Mwacitsanzo , tikadziŵa kuti munthu amene timakonda kapena ifeyo tili ndi matenda oopsa , timamva ngati kuti taphulitsidwa ndi bomba . Timalambila “ iye yekha basi , ” ndipo sitipeputsa malamulo ake ndi mfundo zake zolungama . — Mat . Kodi tili ndi ciyembekezo cotani cakuti akufa amene ali gone m’manda adzakhalanso ndi moyo monga mmene Lazaro ndi mwana wamkazi wa Yairo anacitila ? Zimene tingaŵelenge m’cinenelo cacilendo , sizingatifike pamtima ngati mmene zingakhalile tikaŵelenga m’cinenelo cathu . Kodi Barizilai anaonetsa bwanji mzimu wodzicepetsa ? Kodi tiphunzilapo ciani pa zimene zinacitikila angelo amenewa ? Mboni za Yehova zimadziŵika bwino ndi nchito yao yolalikila . Ndimasinkhasinkha cilamuloco tsiku lonse . M’malomwake , anauza ophunzila ake kuti adzalandila madalitso cifukwa codzimana zinthu zina . • “ Yehova ndi wolungama m’njila zake zonse . ” — Salimo 145 : 17 . Zimenezi zinacititsa kuti Yesu akhale ndi zifukwa zambili zokondela Atate wake . Zimenezi n’zimene Mulungu wamphamvuyonse ananena kupyolela mwa mneneli wake wakale Ezekieli , kuti : “ Mitundu ina ya anthu idzadziŵa kuti ine ndine Yehova . ” ( Ezek . Kodi mphunzitsi angacite bwanji kuti akonzekeletse mtima wa wophunzila ? Patapita nthawi analeka kucita zamizimu . Pambuyo pa miyezi ingapo , anakonza cikwati cake kuti cikhale cogwilizana ndi Malemba , ndipo anakhala wolambila Yehova , Mulungu wamtendele . Yosimbidwa ndi mng’ono wake Samuel Ruiz - león Arroyo Ganizilani za m’bale Walter J . Ndipo m’Baibo muli zitsanzo zambili za atumiki a Mulungu amene anapemphela mokweza mau , koma palibe ciliconse coonetsa kuti iwo anayopa kuti Mdyelekezi akhoza kuwamvela . ( 1 Maf . 8 : 22 , 23 ; Yoh . 11 : 41 , 42 ; Mac . Madalitso ocokela kwa Yehova amenewa amatilimbikitsa kwambili mwa kuuzimu , ndipo ine ndi Lidasi timaona ngati ndi maloto cabe . Kucokela m’Baibulo pa lemba la Mlaliki 1 : 4 . Ndipo anamuuza ciani ? Kodi anthu amene amatonthoza ena amapeza madalitso anji ? Kodi mwatsimikiza mtima kuyang’anabe pa mphoto ? Anthu ambili a m’dela limeneli ndi aubwenzi ndi okoma mtima . ya July 2015 ikupezekanso pa webusaiti yathu pa www.jw.org . 6 : 10 ) Baibo inanenelatu kuti Yesu ‘ adzapita kukagonjetsa anthu pakati pa adani ake . ’ Mfundo ya m’Baibo imene ingatithandize ipezeka pa 2 Akorinto 6 : 14 , 15 . Mungaonenso Salimo 37 : 29 ; ndi 2 Petulo 3 : 13 . Zinthu zofanana ndi zimenezi zingaticitikile ngati tiŵelenga zofalitsa zimene analembela anthu onse . Eliya anatopa kwambili ndi kutentha kwa dzuŵa , ndipo anakhala pansi pa mthunzi ndi kuyamba “ kupempha kuti afe . ” — 1 Maf . 17 : 17 - 24 ; 2 Maf . 4 : 32 - 37 ) Ndipo nthawi ina munthu wina anauka pamene thupi lake linaponyedwa m’manda ndi kukhudza mafupa a Elisa . Kukali zaka pafupi - fupi 200 mfumuyo ikalibe kubadwa , mneneli waciheberi dzina lake Yesaya anatomolelatu dzina la mfumu imene idzagonjetsa mzinda wamphamvu wa Babulo , kuti idzakhala Koresi . Mwacitsanzo , mu 49 C.E . , mzimu woyela unatsogolela bungwe lolamulila kupanga cosankha pankhani ya mdulidwe . Iye anapitiliza kuti : “ Ndimakondwela kuti Yehova anandithandiza kusankha nchito imene imandithandiza kupeza zofunika za paumoyo ndi kucita zinthu za kuuzimu . ” Iye amafuna kuti tizikonda cikhalidwe cathu ndi kusangalala naco . Paulo analemba kuti : “ Aliyense wa ife azikondweletsa mnzake pa zinthu zabwino zomulimbikitsa . ” “ Cikhulupililo . ” Kwa mawiki angapo , n’nali kuseŵenza usiku . Tinali kupulinta kapepa kauthenga kokamba za cizunzo cimene anthu a Yehova anali kukumana naco ku Canada . 32 : 4 ) Kodi tiyenela kucita ciani zimenezi zikaticitikila ? Kodi sikukucititsani kukhulupilila kuti Mulungu ali na mphamvu zopanda malile ? Iye anati : “ Patapita nthawi yaitali conco , n’nayamba kuganiza kuti akulu sanganipatsenso thandizo lina , koma kunicotsa cabe mu mpingo . Ndipo “ kungoŵelenga nkhani zocititsa cidwi zokhudza kukoma mtima , kumathandiza anthu kukulitsa khalidwe la kupatsa . ” 3 : 20 ) Tangoganizani ! Mulungu angacite “ zazikulu kwambili , ” osati cabe zazikulu . John anayamba kuphunzila Baibo ndi Mboni za Yehova , ndipo anatsimikiza mtima kuyamba kutumikila Yehova . Kodi tikudziŵa bwanji zimenezi ? ( 1 Maf . 19 : 4 ) Anthu amene sanakumanepo ndi mavuto amenewa angaone kuti zimene Eliya anapempha ndi “ zopanda pake . ” Komanso ndimanyadila azipongozi anga aŵili , Stephanie ndi Racquel , ndipo ndimawaona ngati ana anga aakazi . ( Yer . 52 : 8 - 11 ) Inde ! TSAMBA 19 • NYIMBO : 91 , 11 Inde , ndife otsimikiza mtima , malinga ngati Yehova alola , kukhala “ zinthu zonse kwa anthu osiyana - siyana . ” ( Aheberi 11 : 6 ) Zimenezi zingaoneke zopepuka . Nkhaniyi idzatithandiza kumvetsetsa cifukwa cake timakamba kuti Mboni za Yehova ndizo zokha padziko lapansi zimene zikukwanilitsa ulosi wa Yesu wa pa Mateyu 24 : 14 . NYIMBO : 135 , 144 ( Ŵelengani Yakobo 4 : 7 . ) 3 , 4 . ( a ) N’ciani cimene tifunika kudziŵa kuti timvetse fanizo la nkhosa ndi mbuzi ? Kuganizila kwambili zinthu zimene munali kucita kale kungakufooketseni ndi kukulepheletsani kucita zimene mungakwanitse . Kodi kuganizila phindu la kukhala wokhulupilika kumatithandiza bwanji ? Si cocokela m’Baibo , koma cinayambila ku zipembedzo zakale zacikunja ndi nzelu za anthu . Zimenezi zikacitika , makolo okalamba ndi ana ao ayenela kukambilana za thandizo limene lingakhale bwino ndiponso limene angakwanitse . Ganizilani nchito yokondweletsa imene tidzakhala nayo , yokonza dzikoli kukhala Paradaiso ndi kumanga nyumba zathu ndi za okondedwa athu . ( Mat . 11 : 1 ) Nafenso tingathandize ophunzila Baibulo kukhala alaliki aluso . ( 2 Mbiri 5 : 13 ; 33 : 4 ) Ngakhale n’conco , m’Baibulo muli mfundo zimene zingatithandize kudziŵa mmene tiyenela kuonela malo athu olambilila ndi mmene tiyenela kuwagwilitsila nchito . 1 : 21 - 23 ) Davide sanasunge cakukhosi . Koma kodi Baibo imakamba ciani pankhani imeneyi ? Kodi mungaŵelenge vesili ? Tsiku lililonse ndikamaganizila pa zinthu zabwino zimene wandicitila , ndimaona kuti ndi mwai waukulu kudziŵika ndiponso kukondedwa ndi Atate wathu wakumwamba amene amatiteteza . Mkazi wake atanamizidwa , anamusonkhezela kupanga cosankha coipa ngako , cimene cinapangitsa kuti ataye mwayi wokhala m’Paradaiso , ndipo m’kupita kwa nthawi anafa . * Mlongo wina analemba kuti : “ Timayembekezela mwacidwi nthaŵi ya Cikumbutso . Mulungu amatambasula ‘ dzanja lake lamanja lacilungamo ’ kwa inu . 18 : 21 ) Eliya anadzudzula anthuwo cifukwa colephela kupanga cosankha . Ungayese kuitsiliza m’miyezi 12 cabe . Nao na Jumpei 2 : 13 , 14 , 19 - 23 ) M’macaputa oyambilila a Uthenga Wabwino wa Mateyu , dzina la Yosefe limachulidwa ka 9 , koma la Mariya limachulidwa ka 4 cabe . Conco , sititengako mbali pa nkhondo ndi ndale za m’dzikoli . N’ciani cimacitika ngati tilola cikondi kutsogolela maganizo na mtima wathu ? Pa zamoyo zonse zimene Mulungu analenga padziko lapansi , anthu analengewa mwapadela kwambili . 6 : 34 ; 7 : 6 , 13 ) Iwo amacita cidwi akadziŵa kuti amene analankhula mauwa ndi Yesu Kristu . Nkhani Yofunika Kwambili 3 Iyai — Yosefe sanabise mkanjo wake . — Luka 11 : 33 . MALOTO A YOSEFE Anthu a m’zipembedzo zambili amakamba kuti amalalikila uthenga wa Yesu . Tikawaphunzitsa na kuwalimbikitsa mwa njila imeneyi , iwo adzayamba kuonetsa ena cidwi ndi kutsogoza maphunzilo a Baibulo awo - awo . Tingagwile nchito pamodzi ndi Wotiumba wathu mwa kuthandiza abale ndi alongo kukula kuuzimu . Koma zimenezi zingatheke ngati timvela malamulo ake . ( Yes . 7 : 9 ; Yoh . 10 : 16 ) Mukufuna kudzakhala ndi moyo kwamuyaya m’Paladaiso , ndipo mumakhala ndi cimwemwe mukaganizila zimene Baibulo limanena ponena za mmene umoyo udzakhalila padziko lapansi . Anadziŵa kuti , mofanana ndi Aisiraeli , iwonso tsiku lina adzaleka kukhala m’kampu . — 2 Akor . Kodi mungapeze mayankho ake ? ( Luka 14 : 28 - 30 ) Tikuyamikila kwambili abale ndi alongo amenewa cifukwa ca zimene amacita . Pa nthawi imene Inoki anabadwa , anthu anali kucita zoipa . Ndikakumbukila zimene ndakumana nazo pa umoyo wanga , ndimayamikila Yehova cifukwa condisamalila nthawi zonse . Kodi mwamunayo na banja lake anatenga sitepi yanji ataphunzila coonadi cokhudza Yesu ? Citsanzo cake ndi cofunika kwambili kwa ife . ( Aroma 7 : 14 , 15 ) Izi zionetsa kuti panali zinthu zina zimene Paulo anaona kuti anali macimo zimene anali kulimbana nazo . Baibo imati : “ Pamene anali kunenedwa zacipongwe , sanabwezele zacipongwe . . . , koma anali kudzipeleka kwa iye amene amaweluza molungama . ” M’malomwake , aloleni kuti adzionele okha mmene kutsatila mfundo za Yehova kwakuthandizilani . ( Onani kamutu kakuti , “ Mmene Mulungu Adzakwanilitsila Cifunilo Cake . ” ) ( Mac . 7 : 8 ) Cifukwa ca njala , Yakobo ndi banja lake anapita kukakhala ku Iguputo . Yosefe , mmodzi wa ana ake , anali kumeneko ndipo anali woyang’anila cakudya , ndiponso munthu wodalilika kwa Farao . ( Gen . 19 : 26 ) Patapita nthawi , Mariya anapezeka ku Yerusalemu pamodzi na ophunzila ena , patatsala masiku angapo kuti ophunzilawo adzozedwe na mzimu woyela pa Pentekosite . ( Mac . ( b ) Kodi mudzapindula motani ngati ‘ mufuna - funa Ufumu coyamba ’ ? ( a ) Ndi mfundo ziŵili ziti zimene tikuphunzila m’fanizo la matalente ? ( Chivumbulutso 11 : 15 ) Ufumu umenewo ndi boma lenileni limene lidzabwezeletsa Paradaiso padziko lapansi . Onse lomba anali atakhala ku thebulo , kuyembekezela cakudya . Margaret anabweletsa cakudya na kuciika pa thebo . Ganizilani mmene Satana anaseŵenzetsela nyambo yake pokopa gulu la angelo anzake . Ngakhale kuti sitidziŵa mmene zinthu zidzakhalila pa umoyo wathu m’dziko latsopano , tiyenela kuuzako ena zimene timafuna kudzacita panthawiyo . Timayamikila kwambili abale na alongo amene amacita khama kuvala bwino ndi kusunga makhalidwe abwino . Komabe , sitiyenela kuleka kulimbana ndi zofooka zathu . — Miyambo 4 : 23 . Ngati timakonda Mulungu , kodi misonkhano tidzaiona motani ? Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Tiyeni tiganizilane . ” M’NTHAWI za m’Baibulo , anthu anali kulandila malangizo a Yehova m’njila zosiyanasiyana . 1 : 18 - 25 . Yesu anali kusunga ndevu , potsatila cikhalidwe ca Ayuda mosiyana ndi Aroma . Acipembedzo , andale , otsatsa malonda , ndiponso zinthu zimene amagwilitsila nchito kufalitsa uthenga wao zonse zimacilikizidwa ndi “ mulungu wa nthawi ino , ” Satana Mdyelekezi . ( 2 Akor . 4 : 4 ; 1 Yoh . 9 : 9 ) Ndiye cifukwa cake Baibulo limalimbikitsa okwatilana kuti : “ Musamanane , [ mangawa a mucikwati ] kupatulapo ngati mwagwilizana kuimitsa kaye mangawawo kwa nthawi yodziŵika . ” ( Yobu 38 : 4 , 7 ; Akolose 1 : 15 ) N’zoonekelatu kuti poyamba analiko yekhayekha . Ngati mkazi wanu ndi ana anu aona kuti mukuyesetsa kukonza zinthu , io adzazindikila kuti mumawakondadi . Ngakhale kuti zinali zovuta kupanga masinthidwe amenewa , banjali limaona kuti ndi mwai kugwila nao nchito yofunika kwambili imeneyi . Inapulumuka ( 1 ) kuti isawole cifukwa ca zimene anali kulembapo , monga gumbwa na zikopa ( zikumba ) za nyama ; ( 2 ) kwa anthu andale ndi acipembedzo amene anafuna kuiwononga ; ndi ( 3 ) kwa anthu ofuna kusintha uthenga wake . — wp16.4 , mapeji 4 - 7 . 11 : 17 - 19 ) Zimenezi zinalimbitsa Mose kukonda Mulungu amene anali kucitila cifundo Aheberi ndi anthu onse . Motelo , zimene omasulilawo analemba zinakhala mbali ya Baibulo limene tili nalo masiku ano . Koma ngati mukufunadi munthu wokwatilana naye , Mulungu amadziŵa bwino mmene angakhutilitsile zokhumba zanu . — Sal . N’cifukwa cake n’napezeka m’nyumba yozizila ya pa famu imene nachula poyamba paja . N’nali kuyembekezela kubatizika . 6 : 44 ) Yehova amatitsimikizila kuti amatikonda ndipo amatithandiza kupilila pom’tumikila . Anawalilila ndi kuwacondelela koma io anamunyalanyaza . ( Amosi 5 : 15 ) Koma kodi tingacite bwanji zimenezi ? ( b ) N’ciani cionetsa kuti angelo ndi adongosolo ? ( Genesis 20 : 12 ) Ngakhale kuti ukwati waconco si woyenela masiku ano , n’kofunika kuganizila mmene zinthu zinalili kalelo . Yosimbidwa ndi Antoine Touma Ndipo inanena kuti kumatanthauzanso “ kukhulupilila kuti anthu a mitundu ina ali ndi maluso ndiponso makhalidwe osiyana ndi ena , komanso kuti mitundu ina ndi yapamwamba kuposa ina . ” Pa Pentekosite wa mu 33 C.E . , mtumwi Petulo anakamba kuti mau amenewa anali kukamba za Yesu pamene anati : “ [ Davide ] anaonelatu zapatsogolo ndi kunenelatu za kuuka kwa Kristu . Ananenelatu kuti iye sanasiyidwe m’Manda , komanso kuti thupi lake silinavunde . ” — Mac . 2 : 23 - 27 , 31 . Panthawiyo , mwina iye anali kudziimba mlandu akaganizila mau aukali amene anakamba m’mbuyomo okhudza Asamariya . — Mac . 8 : 14 , 25 . N’nayamba kudzitangwanitsa mwa kucita zinthu zina . 3 MBILI YANGA ​ — Napindula Cifukwa Coyenda ndi Anthu Anzelu Tingakambe kuti imfa yake inali yodabwitsa kwambili komanso yocititsa cidwi kuposa umoyo wake . M’maiko ena boma limathandiza okalamba mwa kupeleka mapenshoni ndi kukonza mapulogalamu othandiza osauka . Tsopano tiyeni tikambilane mbali zitatu za umoyo wathu zimene tifunika kusamala nazo kuti tipitilize kukonda kwambili Khristu ndi zinthu zauzimu . Mbali zimenezi ndi nchito yakuthupi , zosangulutsa , na cuma . Mu 1916 , iye anakhazikitsanso kabungwe ka anyamata kochedwa Wolf Cubs ( kapena Cub Scouts . ) Inde , tifunika kukhulupilila kuti Yehova , “ Woweluza wa dziko lonse lapansi , ” nthawi zonse adzacita zinthu mwacilungamo cifukwa “ njila zake zonse ndi zolungama . ” — Gen . ( Genesis 1 : 27 ) Zimenezi zitanthauza kuti tikhoza kuona kuti iye amatikondadi , ndipo ifenso tikhoza kumuonetsa kuti timam’konda . Mau a Paulo aonetsa kuti iye anagwila mau a malemba ena . Anthu amagwilitsila nchito mabwato aang’ono akafuna kuyenda ulendo waufupi . Kodi citsanzo ca Mfumu Sauli cili ndi cenjezo lotani kwa ife ? Komabe , Mulungu amaona kuti malonjezo amene timapanga ni opatulika , ndipo ni osasinthika cifukwa amalowetsamo lumbilo lakuti munthu adzacita zinthu zina kapena sadzacita . ( Gen . 14 : 22 , 23 ; Aheb . Khalidwe lathu lingaonetse kuti sitilemekeza Mulungu ( Onani ndime 7 ndi 8 ) Yesu sanali kulakalaka kulemekezedwa na atsogoleli acipembedzo kapena andale a m’nthawi yake . Sitifunika kuganiza kuti okhawo amene ali na nyumba zapamwamba ndiwo ayenela kuthandiza , cifukwa iwo angakhale kuti anacitapo kale zimenezi nthawi zambili . Pamene tiganizila mmene tinadziŵila Yehova , tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ubwenzi wanga ndi Mulungu ukupita patsogolo ? Tingacite ciani kuti tikhalebe pamtendele na abale athu ? ( Luka 1 : 26 - 56 ) Luka analembanso zimene Simiyoni anauza Mariya zokhudza mavuto amene Yesu anali kudzakumana nawo m’tsogolo . Mwacibadwa , ise anthu sitifuna kudzilanga tekha . Kuonjezela apo , panalinso ma Yehu aang’ono 11 amene munali kugona anthu aŵili , ndipo anali kukokedwa ndi njinga . Iye anati : “ Akalumbila kucita zinthu zimene kenako zakhala zoipa kwa iye , sasintha malingalilo ake . ” Sitidzakamba zabodza kwa io , kuwabela , kapena kuwacitila ciliconse cosemphana ndi mfundo za Yehova ndi malamulo ake . Ali mu mzinda wa Filipi , anthu otsutsa anawaponya m’ndende . Ngati ndinu wokonzeka kukhululukila ena , mudzaonetsa kuti mumagwilizana ndi cilungamo ca Yehova . — Ŵelengani Mateyu 6 : 14 , 15 . Ndipo n’cifukwa cake nthawi zonse popemphela ndimachula dzina la Yesu . Mwacikondi cake , Yehova anatipatsa mfundo zimene tingazigwilitsile nchito mogwilizana na cikumbumtima cathu cophunzitsidwa Baibo . Nkhanizi zifotokoza mmene tingacitile zimenezi . KODI ANTHU NDI AMENE AMACITITSA ? Molingana ndi wolemba Salimo 147 , kodi si zoona kuti tili na zifukwa zambili zofuulila kuti “ Tamandani Ya ! ” Conco , mwamuna wakeyo anasiya nchito . Komanso , ‘ kuipa kwa anthu kunaculuka padziko lapansi ’ ndipo “ malingalilo onse a m’mitima ya anthu anali oipa okha - okha nthawi zonse . ” — Gen . Tingaonetse bwanji kuti timalemekeza misonkhano yathu ? Msilikali winanso ananipatsa cakudya cimene iye analandila kuti adye . Timacita zimenezi cifukwa timamvela mau a Yesu akuti Akristu ‘ sayenela kukhala mbali ya dziko . ’ N’nali kudzimva kuti nikudziŵikitsadi dzina la Yehova . ” Kodi aja amene akukalamila kukhala oyang’anila ayenela kudela nkhawa monga mmene Fernando anacitila ? ( Aroma 5 : 12 , 16 ) Lemba la Aroma 5 : 18 limati : “ Mwa ucimo umodzi anthu kaya akhale amtundu wotani anaweluzidwa kukhala ocimwa . ” Kuyambila nthawi imeneyo , tinali kusangalala poceza pamodzi ndi kukambilana za Mulungu wathu wokondedwa , Yehova , ndi Mau ake . 28 : 19 , 20 ) Kodi inu ndi mpingo wanu mungathandize makolo a atumiki anthawi zonse amene angafunikile thandizo ? Mwacionekele , kusinkhasinkha mavesi a m’Baibulo kunawonjezela cidziŵitso canu . Zimenezo zinacititsa kuti mukhale ndi cuma cambili ca kuuzimu . Yehova anatikonda kwambili cakuti anatipatsa mphatso yamtengo wapatali . Ganizilani za mtumwi Paulo . Njila imodzi ni kufufuza mau ena a m’Baibo amene angatiunikileko mmene anali kuonekela . Masiku anonso , anthu okhawo amene Yehova amawaona kuti ni olungama monga Nowa , Danieli , na Yobu , ndi amene adzaikidwa cizindikilo kuti akapulumuke pa mapeto a dziko loipali . ( Chiv . Anthu okonda zinthu zakuthupi cimawavuta kuika zinthu zauzimu patsogolo . N’taphunzila Cipwitikizi kwa caka cimodzi , n’naikidwa kukhala woyang’anila dela . Koma mulimonse mmene zinthu zidzakhalile tidzafunika kukhala oyamikila ndiponso okhutila pamene tikugonjela ku ulamulilo wabwino wa Yehova . Mwacitsanzo , timaphunzila za zinthu zoipa zimene zimapezeka pa Intaneti , kuipa kokonda ndalama , za ciwelewele , mafilimu a ciwawa , mabuku ndi maseŵela oipa a pa kompyuta . Aliyense amene ali ndi mtima wofunitsitsa apeleke kwa Yehova . ” ( Eks . ( Luka 16 : 11 ) Mlongo wina amene kaŵili - kaŵili amacita zopeleka zocilikizila nchito ya Ufumu , anafotokoza madalitso amene wapeza . Anati : “ Cifukwa cokhala wowoloŵa manja , umoyo wanga wasintha ngako m’zaka zapitazi . Baibulo limaonetsa kuti anali kumvetsela mosamala zinthu zimene anali kumva , makamaka zinthu zokhudza Yehova . N’cifukwa ciani amalephela kuona kuti zinthu zimene zikucitika m’dzikoli zikukwanilitsa ulosi wa m’Baibo monga mmene atumiki a Mulungu akhala akulalikilila kwa zaka zambili ? Koma anali kudziwa kuti cinthu cinacake capadela cokhudza Ufumu wa Mulungu cidzacitika m’caka ca 1914 . Ndiyeno , ophunzila Baibo ndi ena ozilala nawonso anayamba kufika . Ine ndi mkazi wanga tinaona kuti Baibulo limatithandiza kukhala ololela . Iye ndi amene anaona zabwino mwa inu ndipo anafuna kuti mum’dziŵe . Ulamulilo wa Soviet Union unaphatikizapo cigawo ca Siberia , kumene adani a Boma anali kutumizidwa monga akaidi . Ataona bwenzi lake Mariya ndi anthu ena akulila imfa ya Lazaro , Yesu “ anagwetsa misozi . ” 7 : 23 - 25 ) Komabe , Yehova asanam’patse nchito imeneyo , Mose anafunikila kuphunzila zambili . 6 : 33 ; 24 : 14 . Atanditsekela kacitatu , anandiuza kuti ndingacoke ngati ndalemba mau awa : “ Ndikucoka cifukwa cakuti ndifuna kutumikila Satana osati Mulungu . ” Ifenso tingacite bwino kutengela citsanzo cawo cabwino . Ndani amene akulalikila uthenga wabwino wa Ufumu masiku ano ? 32 Mlozela nkhani wa Nsanja ya Mlonda wa 2014 19 : 5 - 8 , 15 - 19 . Ngati tipanga zosankha zimene zimakondweletsa Yehova , tidzamuyandikila , ndipo iye adzatikonda ndi kutidalitsa . [ Mau apansi ] Macenjezo ena othandiza mukhoza kuwapeza m’nkhani za m’magazini otsatilawa : Nsanja ya Olonda ya August 15 , 2011 , tsamba 3 mpaka 5 pa nkhani yakuti “ Tiyenela Kugwilitsa Nchito Intaneti Mwanzelu . ” Wamasalimo anati : “ Ndi bwino kuyamika inu Yehova . . . Komanso mlongo Anna Gardner anakamba kuti “ mtenje unanjenjemela mwamphamvu cifukwa abale na alongo anaomba m’manja kwambili na cisangalalo . ” 44 : 22 . Kutsanzikana na alendo kunatanthauza kuwapatsa zinthu zilizonse zofunikila paulendo wawo kuti akafike kumene akupita . N’zoonekelatu kuti Gayo anali atacitapo kale zimenezi kwa alendo . ( b ) Kodi tiyenela kukumbukila ndani ngati pali zinthu zimene zingaticititse kuopa anthu ? Aliyense wokhulupilila Mulungu anali kumuona kuti ni mbuli . ” Conco , iye anauza Mose ndi Aroni kupita kwa Farao kukamuuza kuti : “ Yehova Mulungu wa Isiraeli wanena kuti , ‘ Lolani anthu anga apite m’cipululu kuti akacite cikondwelelo . ’ ” — Eks . Baibulo limanena kuti : “ Kukonda Mulungu kumatanthauza kusunga malamulo ake , ndipo malamulo akewo ndi osalemetsa . ” — 1 Yoh . 5 : 3 . Nthawi zonse , Yehova amakhala wokonzeka ‘ kuthandiza anthu ofatsa . ’ Iwo sapatsidwa ndalama cifukwa colalikila , koma amakhala okondwa ngakhale kuti amaseŵenzetsa ndalama zao pogwila nchito imeneyi . KODI mungakwanitse kuŵelenga Baibo ya Ciheberi ? Cifukwa cakuti nthawi zonse , anali kuona kuti ubwenzi wake ndi Yehova ndiwo cinthu cofunika kwambili . Ndiyeno Abisai anauza Davide capansipansi kuti : “ Ndilole conde , ndimubaye ndi kumukhomelela pansi ndi mkondo kamodzi kokha , sindicita kubweleza kaŵili . ” 3 : 19 ) Ise timadziŵako “ kambali kakang’ono cabe ka zocita zake , ” ndipo “ timangomva kunong’ona kwapansi - pansi kwa mau ake . ” Tinali kuyenda ndi boti kukaceza ndi anthu tsiku lonse , ndipo tinali kuwaitanila kunkhani ya Baibulo . ( Mateyu 6 : 6 - 8 ) Tikamapemphela nthawi zonse kwa Mlengi wathu tidzakhala paubwenzi wolimba ndi iye . Yehova Mulungu analonjeza kuti adzadalitsa atumiki ake okhulupilika . Komabe , ine ndinavutika kuleka ngakhale nditayesa kucita zimenezo pafupifupi maulendo 6 . ” Nkhani ya Yobu ingatithandize kukhala na maganizo oyenela ndi kutitonthoza . N’cimodzimodzi ndi Nowa . Yehova anaonetsa cimene cinasoŵekaco pamene anakamba kuti : “ Si bwino kuti munthu akhale yekha . Wina anali kutumikila monga mmishonale ku Paraguay , ndipo wina anali kutumikila ku likulu ku Brooklyn , New York . Nkhaniyo inakamba kuti sizinali kudziŵika bwino kuti tuzipangizo tumenetu tumaseŵenza bwanji . Kodi ndinu okonzeka ndi ofunitsitsa kulimbikitsa abale anu ? Ngati Carin akanatumiza ana ake kwa makolo ake kuti aŵalele , pakanakhala zotsatilapo zoipa . Matthew anati : “ Ndinavutika kuti ndiphunzile cinenelo ndipo zinali zovuta kukambilana ndi anthu nkhani za m’Baibulo . ” Zondidabwitsa n’zakuti , mphunzitsiyo anali womasuka ndipo anandilola kuti ndikafotokoze cikhulupililo canga pa nkhani ya cilengedwe m’kalasi . ” Kodi tapindula bwanji pa nthawi za mtendele ndiponso pogwilitsila nchito njila zamakono za mayendedwe ? Makhalidwe onse amene takambilana ni ogwilizana kwambili ndi cikondi . NKHANI YA PACIKUTO | NI MPHATSO ITI YOPOSA ZONSE ? ( Mateyu 6 : 8 ) Mfumu ya Isiraeli inavomeleza mfundo imeneyi , ndipo inalemba kuti : “ Ndisananene kanthu , inu Yehova mumakhala mutadziŵa kale zonse . ” Nanga tidzakambilana ciani kuti tipeze yankho yake ? Muzibwelelako kwa onse amene anamvetsela uthenga wa Ufumu . Onani nkhani yakuti “ Kodi ‘ Mungawolokere ku Makedoniya ’ ? ” Koma munthu wauzimu amamvetsetsa mmene Mulungu amaonela zinthu komanso amazindikila njila yoipa ya munthu wakuthupi . Malinga n’zimene Malemba amakamba , makolo ndi amene ali na udindo wophunzitsa ndi kulangiza ana awo . ( Miy . Tiyeni tonse tipitilize kulemekeza kwambili abale okhala ngati amenewa . — Afilipi 2 : 29 . Pemphelo limenelo limachedwa Shema . Shema ni liu loyambilila pa vesi imeneyi m’Ciheberi . Mungacitenso bwino kuwathandiza kuganizila pa mafunso monga awa : ‘ N’cifukwa ciani Baibo imaletsa zinthu zina zimene zimaoneka zokopa ? 20 : 10 , 11 . ( Salimo 31 : 5 ; Malaki 3 : 6 ) Ponena za Mulungu Yesu anati : “ Mau anu ndiwo coonadi . ” 26 : 52 ) Sitilola kunyengeleledwa ndi dziko la Satana kuti titengemo mbali m’ndale . ( 2 Akor . Nsembe zathu zacitamando kwa Mulungu zimacokela pansi pamtima cifukwa timam’konda . Iye anali “ mwana wa Mulungu ” ndipo analengedwa m’njila yakuti azikwanitsa kutengela makhalidwe a Mulungu . — Luka 3 : 38 . Anafunikila kukulitsa makhalidwe monga kudzicepetsa , kuleza mtima , kufatsa , ndi kudziletsa . Conco , mungathe kukhala na cimwemwe coculuka ngati nthawi zonse mumapempha thandizo la mzimu wa Yehova na kusinkha - sinkha Mau ake ouzilidwa na mzimu . — Sal . Ofalitsa a kum’mwela kwa dziko la Chile akuyenda m’mbali mwa mtsinje wodutsa m’nkhalango na m’mapili a Andes okhala ndi sinowu ( snow ) pamwamba pake . Ngakhale kuti mwina ise sitinacitilidwepo nkhanza zaconco , zocita za anthu oipa zimatikhudza ndithu . Mofanana ndi Paulo , sitikaikila ngakhale pang’ono kuti Yehova adzatithandiza kupilila mpaka mapeto . Afunika kupanga cosankha monga banja limene lifuna kukondweletsa Mulungu na kukhala na cikumbumtima coyela pa maso pake . — Yelekezelani na 1 Timoteyo 1 : 18 , 19 ; 2 Timoteyo 1 : 3 . M’nkhani yotsatila tidzakambilana mapempho amenewa . Kodi inu mumayesetsa kutengela citsanzo ca Yesu mwa kukhala wokonzeka kucitila cifundo anthu amene afunika thandizo ? Kodi tifunika kudandaula ngati ana athu afuna kukamba na ise ? Mofananamo , Yesu anafuna kuteteza anthu a mu Yerusalemu mwauzimu . Kodi mumaona pemphelo kukhala cabe njila yokuthandizani kukhala ndi maganizo oyenela ? Patapita nthawi , Davide anaitanidwanso . Anthu onsewo anafa mosasamala kanthu zakuti anali anthu otani . Ngakhale Abulahamu analila imfa ya Sara . Mulungu sanaganize kuti , ‘ Popeza Yesu n’naseŵenza naye kwa zaka zambili - mbili kuno kumwamba , palibe cifukwa comuyamikilila na kumulimbikitsa pamene ali pa dziko lapansi , ayi . ’ 48 : 17 , 18 ) Ngati tiganizila mozama mfundo za m’Baibo na kuzilola kutifika pa mtima , tingawongolele cikumbumtima cathu . Kenako , Rehobowamu anapita ku Sekemu , dela la kumpoto kwa Yerusalemu , kuti akamulonge ufumu . Nchito yolalikila ndi yaikulu ndipo ifunika kucitidwabe . Mumpingo wathu wa ku Adelaide munali Akhristu odzodzedwa acikulile okwana 12 . Kodi alendo tingawaonetse bwanji kukoma mtima ? 3 : 18 ) Muyenela kuwaphunzitsa zinthu zogwilizana na msinkhu wawo ndiponso luso lawo lomvetsa zinthu . Baibo imasiyanitsa kudzicepetsa ndi kudzikweza . 17 : 26 ) Cifukwa ca ici , tonse ndife amodzi popeza tinacokela kwa kholo limodzi loyambilila , Adamu . Mzimayi wacitsikana , Isabella , anakamba kuti : “ Niganiza kuti kuzengeleza ise n’cakubanja , cifukwa atate nawo niwozengeleza kucita zinthu . Conco Yehova anamuuzilatu Baruki kuti maganizo ake anali olakwika ndipo anafunika kusintha . N’natsatila malangizo anzelu opezeka pa Afilipi 4 : 6 , 7 , amene amati : ‘ Musamade nkhawa ndi kanthu kalikonse , koma . . . zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu . ’ ( Yoh . 6 : 66 - 68 ) Mofanana ndi Akhristu anzanga ogontha amene akhala m’coonadi kwa zaka zambili , naphunzila kukhala woleza mtima . N’cifukwa ciani tingakhale ndi cidalilo cakuti Yehova adzatidalitsa ngati timacita zabwino ? Ciliconse cimene Yehova anapanga padziko lapansi , cimapindulitsa anthu ndi nyama ( 1 Sam . 3 : 19 ) Popeza kuti io amakonda coonadi , anthu ena amatilemekeza . Masiku ano , anthu oipa amangocita zinthu monga vilombo kapena viŵanda . ( Yak . 19 : 7 ) M’kupita kwa nthawi , angapatsiwenso maudindo . Anadziŵa kuti Mulungu amasamalila nthawi zonse . 6 : 20 . Akristu anapindula ndi miseu yabwino ya Aroma . ( a ) Kodi Yesu anaikidwa liti kukhala Mfumu ? N’cosankha citi cimene Aisiraeli anafunika kupanga ? Nanga n’cifukwa ciani iwo analephela kusankha mwanzelu ? 1 , 2 . ( a ) N’ciani cimene cikuthandiza Akhristu acicepele kupambana pa nkhondo yolimbana na ziŵanda ? Cinanso , ngati mlandu unali na mboni , zinali kufunika kukhala zosacepela ziŵili kuti atsimikizile kuti munthu anaphadi mnzake mwadala . — Num . M’fanizoli , Yesu sanali kutanthauza kuti ena amene ali m’gulu la kapolo wokhulupilika ndi wanzelu adzakhala oipa . Onse amene amamvela “ cilamulo ca Kristu ” afunika kulalikila . Nchito yao ndi kufotokozela Bungwe Lolamulila mfundo zina zofunika ndi kupelekapo malingalilo ao . Kodi Yehova anam’patsa cilango canji Sebina ? Ndimakonda kuphunzila za mbili yakale kuti ndidziŵe mmene anthu apitila patsogolo . Iye anati , “ Cinthu cokondweletsa ngako kwa ine ni kuona ana anga auzimu ‘ akupitirizabe kuyenda m’coonadi . ’ ( Genesis 1 : 31 ; 2 : 15 - 17 ) Colinga cake cimeneci sicinasinthe . 6 : 24 ; Eks . Pamene n’nacokapo , Mary anali kulalikila m’gawo lamalonda la Cipwitikizi , mmene anthu anaika maganizo awo onse pa kufuna - funa ndalama basi . Mouzilidwa , Enoki ananenelatu kuti Yehova adzabwela “ ndi miyandamiyanda ya oyela ake , kudzapeleka ciweluzo kwa onse , ndi kudzagamula kuti onse osaopa Mulungu apezeka ndi mlandu cifukwa ca nchito zao zonyoza Mulungu zimene anazicita mosaopa Mulungu , komanso cifukwa ca zinthu zonse zonyoza koopsa zimene ocimwa osaopa Mulungu anamunenela . ” Yehova , ni Mulungu wa coonadi . Posakhalitsa , tinayamba kulandila atumiki amadela ( amene lomba timati oyang’anila dela ) kunyumba kwathu . Cifukwa cakuti nthawi zambili akazi sanali kuwaŵelengela pa mzela wobadwila . Zidzatithandizanso kudziŵa mmene tingadzitetezele ku njila zake zacinyengo . Kodi tingacite ciani kuti tisafooke ndi zimene timaona mu galasi imene ndi Mau a Mulungu ? Poyamba iye anacita mantha . Mofanana ndi abale ndi alongo okwana 17 amene anasamukila ku Ghana , ofalitsa ambili “ adzipeleka ndi mtima wonse ” cifukwa cokonda Yehova . Mose “ anaona kutonzedwa kwake monga Wodzozedwa kukhala cuma coculuka kuposa cuma ca Iguputo . ” Iye analola “ khamu la anthu a mitundu yosiyanasiyana ” amene sanali Aisiraeli , kuphatikizapo Aiguputo , kutsatila anthu ake pamene anawatulutsa mu Iguputo . PACIKUTO : Woyang’anila dela ndi apainiya apadela amayenda pa bwato mu mtsinje wa Amazon . Kodi muganiza n’ciani cimene Mulungu wacita cimene cionetsa kuti amakukondani ? Iye anakamba kuti anali kudziona monga wacinyengo cifukwa anali kukonda kuchova njuga . Ni mfundo yofunika iti imene Yesu anaphunzitsa pankhani yosankha zinthu zoyenela kuika patsogolo ? Conco , pofuna kutithandiza kuti tipewe kucita zolakwa zazikulu , Yehova watipatsa zitsanzo zoticenjeza . 32 : 1 , 2 , 17 , 18 . Kodi ndine wotsimikiza kuti nkhani imeneyi ndi yoona ? ( Mika 6 : 8 ) Conco , nthawi zonse tikalandila udindo watsopano , tifunika kuganizila mwa pemphelo zilizonse zimene Yehova akutiuza kupitila m’Mau ake na gulu lake . Izi zili conco , cifukwa cakuti anthu ndi nyama anapangidwa ndi Mlengi kuti azikhala padziko lapansi . ( Ŵelengani Chivumbulutso 20 : 12 . ) Tifunika kucita ciani kuti zolakwa zathu zikhululukidwe ? Komanso ngati mufuna , mungaŵelenge Baibo motsatila mitu ya nkhani kapena motsatila ndondomeko ya mmene zinthu zinacitikila . Conco , zinthu zoipa zikacitika , ndani amene tiyenela kuimba mlandu ? Mzimu woyela unayenelanso kutsanulidwa pa aja amene anali kudzakhala “ olandila coloŵa anzake a Kristu . ” Ndiyeno , ganizilani bwino mphatso imene mungamupatse kuti im’thandize pa cosoŵa cake . Koma tsopano , Nsanja ya Mlonda imapezeka m’zinenelo zoposa 240 . Ndipo m’zinenelo zambili magazini imeneyi imatulukila pamodzi ndi ya Cingelezi . Nkhani yotsatila idzafotokoza zimenezi . Ponena za vinyo , Yesu anakamba kuti : “ Kapu iyi ikutanthauza pangano latsopano pamaziko a magazi anga . ” Nafenso tiyenela kucita cimodzimodzi . Angelo ni angwilo , koma anthu amene iwo anali kuthandiza sanali angwilo . Lemba la Malaki 3 : 6 , limati : “ Ine ndine Yehova , sindinasinthe . ” 12 Mgwilizano Wokondweletsa pa Cikumbutso Pambuyo pake , Mdyelekedzi adzaonongedwa kothelatu . Tikatelo , Atate wathu wakumwamba adzadalitsa khama lathu . — Akol . Tingagwilitsile nchito mafunso awa podzifufuza : Koma kodi timacita ciani tikapemphedwa kucita zinthu zina zimene ifeyo sitikufuna ? Ponena za mpingo wa ku Yerusalemu Baibulo limati , “ panalibe ngakhale mmodzi wosoŵa kanthu . ” 13 : 4 - 8 . 3 : 2 ) Pamene Yesu anabatizidwa ndi Yohane , Yehova anadzoza Yesu kukhala Mesiya wolonjezedwa ndiponso Mfumu ya Ufumu wa Mulungu yamtsogolo . Kodi lamulo la pa Genesis 2 : 16 , 17 linali n’colinga canji ? Mwina mungakambe kuti zimenezo ‘ n’zosatheka . ’ Satana sanaganize kuti khandalo linali lokongola , losangalatsa ndiponso lamtengo wapatali . ( Nyimbo 6 : 4 - 7 ; 7 : 1 - 10 ) Kenako , Solomo analola mtsikanayo kubwelela kwao . Akatswili odziŵa mbili ya ku Iguputo , Richard Parkinson ndi Stephen Quirke , anakamba kuti : “ Gumbwa amawola mwamsanga ndi kusanduka dothi . Nditacita upainiya kwa kanthawi , ndinafuna kukatumikila ku malo osowa . ( Luka 10 : 25 - 37 ) Kukhulupilila malonjezo a Mulungu ndi kukonda anansi athu , kudzatithandiza kutengamo mbali mokwanila m’nchito yolalikila madzi asanafike m’khosi . “ ANAOLOKA NYANJA YOFIILA ” M’kupita kwa nthawi , iye anadzakhala munthu wofunika kwambili mu umoyo wanga — anakhala mkazi wanga . Koma Mulungu atamveketsa mfundo yakuti Akhristu sayenela kukhala a tsankho , Petulo analalikila Koneliyo , msilikali waciroma . Kodi mungakonde kukhala pakati pa anthu aconco ? ( Yeremiya 30 : 11 ; 46 : 28 ) Iye amayang’ana nkhani yonse , kuphatikizapo zimene sitingamvetsetse . 3 : 18 ) Mwacitsanzo , timaonetsa kuti timakonda Mulungu ndi anzathu mwa kulengeza “ uthenga wabwino wa ufumu . ” ( Mat . Pambuyo pakuti waononga dongosolo loipa la zinthu la Satana padziko lapansi , Kristu ‘ mu ulemelelo wake adzapambana pa nkhondo yake . ’ Kodi mipukutu ya Baibulo yakale imatsimikizila bwanji kuti uthenga wa m’Baibulo unatetezedwa ? Mwamunayo anayamba kusonkhana nthawi zonse , ndipo patapita nthawi yocepa anabatizidwa . Anzanga a m’kilasi amafotokozela anzawo momasuka zimene amacita . “ Yeletsani manja anu , . . . ndipo yeletsani mitima yanu . ” — YAK . Komanso anali kuyembekezela kudzakhala ndi moyo mu “ mzinda wokhala ndi maziko enieni , ” umene ukutanthauza dziko lapansi lolamulidwa ndi Ufumu wa Mulungu . Ganizilani cabe mmene n’namvelela n’tawaona ndi kukhalako nawo pamodzi ! Kucita zimenezi kumafuna khama , ndiye cifukwa cake mtumwi Paulo anati : “ Ndikumenya thupi langa ndi kulitsogolela ngati kapolo . ” ( 1 Akor . Yehova ayenela kuti anacotsa moyo wa Inoki pang’no - pang’ono popanda iye kudziŵa kuti ali kufa . — wp17.1 , mapeji 12 - 13 . 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani Aisiraeli 24,000 analephela kulandila madalitso ? Mosiyana ndi anthu ambili m’dzikoli , amene alibe cikondi , anthu a Yehova amaonetsa cikondi ceni - ceni kwa anthu anzawo . Cifukwa cacikulu n’cakuti zinatsatila citsanzo ndi ziphunzitso za Yesu . Zonse zinali kudzakulila pamodzi kufikila “ mapeto a nthawi ino . ” 17 , 18 . ( a ) N’cifukwa ciani nthawi zonse tiyenela kudya cakudya ca kuuzimu ? Kodi Satana anakamba ciani ponena za ulamulilo wa Mulungu ? Dipo linatsegula khomo kwa ana onse a Adamu okonda cilungamo kuti adzakhale mbali ya banja la Mulungu . Pamene anafika kumalo kocezela mu mzinda wakale wa Betelehemu , anamva njala kwambili ndipo anali ofunitsitsa kudyako zakudya za kumeneko . Acibale ake ndi mabwenzi ake anadabwa kwambili , pamene mwadzidzidzi Smita anadwala ndipo anamwalila mlungu umodzi usanathe . Komabe pamene mapeto akuyandikila , zocitika zonsezi zakhala zikucitika panthawi yovuta imeneyi . Ndi wotani ? ( Yohane 1 : 1 , 14 ) Amachedwanso kuti “ Mfumu ya mafumu ndi Mbuye wa ambuye , ” komanso kuti “ Wokhulupilika ndi Woona . ” Ganizilani citsanzo ca David . Iye anasiya nchito yake ya malipilo apamwamba m’dziko la Mexico , ndi kuyenda kumudzi m’dziko la Costa Rica kukaphunzitsa ena Baibo . ( 2 ) Kukhala wokhutila na zimene Mulungu amatipatsa . Koma ziphunzitso zake zinali zofunika kwambili , cifukwa zili na mfundo zimene zidzathandiza anthu kukhala amtendele ndi ogwilizana kwamuyaya . Ndi mwai waukulu kukhala Mboni ya Yehova yobatizidwa . Baibulo limayelekezela citsanzo cimene Yesu anasiya ndi “ mapazi , ” kapena zidindo za mapazi . Cimene anakanila pempho la Davide sicinali kuopa kuti sangakwanitse udindowo ayi , kapena kungofuna kusangalala ndi kupuma kwake panchito ayinso . N’nayamba kuona kuti palibe amanikonda . Nthawi zina , ana akulu - akulu angazindikile kuti afunika kusamukila mumpingo wa citundu cimene amamvetsetsa kuti akwanitse kutumikila bwino Yehova . Ngati mumaona zinthu moyenela , mudzacita utumiki mwakhama ndiponso mofunitsitsa . Zilizonse zimene ndinali kuphunzila zinali kundithandiza kuona bwinobwino kuti ndifunika kusinthilatu umoyo wanga . 4 : 2 , 3 ) Timadzionela tekha mtendele umenewu tikakhala pa misonkhano yampingo , yadela , ndi yacigawo . Tingapindule bwanji cifukwa cothandiza ena kulimbitsa cikhulupililo cao ? Nthawi zina mwadala tinali kucita zinthu zosokoneza pa phunzilo la banja kuti lisacitike . Tiphunzilapo ciani pa citsanzo ca Davide ? Pokumbukila zimene zinacitika , mnyamatayo anati : “ Ndinacita cidwi kwambili ndi kukoma mtima kwa akuluwo . N’cifukwa ciani tiyenela kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Mulungu ? Pamene Aisiraeli anali kumasulidwa ku Babulo , ena a io anali atadziŵa kale kukamba Ciaramu . Ni mfundo ziti zimene ayenela kuganizila posankha njila za cilezi ? Koma Mulungu anapatsa mtundu wa Aisiraeli lamulo lakuti : “ Mwamuna akapezeka akugona ndi mkazi wa mwiniwake , mwamuna ndi mkaziyo , onsewo azifela pamodzi . ” — Deut . ( Aroma 15 : 4 ) Kucita zimenezi kudzatithandiza kukhala mwamtendele ndi anthu ena . Baibulo limakambanso za kupangidwa kwa mtunda ndi nyanja . Paulo anacita zimenezo mwa kukamba nkhani yolimbikitsa . Yehova anati : “ Tenga Isaki mwana wako mmodzi yekhayo , mwana wako amene umamukonda kwambiliyo , ndipo . . . ukamupeleke nsembe yopseleza . ” ( Gen . Woyang’anila dela wina ku United States anafotokoza kuti anagaŵila Galamukani ! Mabanja ena ‘ amasangalala kwambili ’ ndi kulambila kwa pabanja monga mmene Yesaya anafotokozela ponena za Sabata . — Yes . Kunena zoona , sindinali kuikonda nchitoyi . ( 2 ) Kumasulila uthenga wake liu ndi liu ngati n’kotheka , koma ngati n’zosatheka , kumasulila tanthauzo lenileni la mauwo . Mwacionekele , ana anu adzalemekeza zofuna zanu ndi kucita zonse zimene angathe kuti muzikhala nokha . Tinayamba kutumikila kumeneko mu January 1979 . Koma cifukwa cakuti ndife opanda ungwilo , tingakopeke ndi ciwelewele , monga mmene nsomba zimakopekela ndi nyambo . 64 : 8 . Mwacitsanzo , mlongo wina , mwamuna wake anamuuza kuti azipita mu ulaliki pa masiku amene mwamunayo anamulamula . Cizunzo citafika pacimake m’dziko la Malawi , ife ndi Mboni zina masauzande ambili tinathawa m’dzikoli . 5 , 6 . ( a ) N’cifukwa ciani Yesu anakamba kuti : “ Mudzakhala mboni zanga ” ? Koma ni “ wacifundo coculuka . ” — Aef . Koma ngakhale zinali conco , ndinayesayesa mpaka ndinayamba kukonda Yehova . Ndinaonanso kuti cinacake casintha mwa ine — cikumbumtima canga cinayamba kundivutitsa . 5 : 13 . Mafunso amene anabuka okhudza ulamulilo wa Mulungu , anafunikabe kuyankhidwa . Araceli : Nditangoyamba kuphunzila Baibulo ndi a Mboni za Yehova , ndinali kuwakaikila . ( Yesaya 1 : 18 ) Ndinacondelela Yehova m’pemphelo kuti andithandize kuleka khalidwe langa . 9 , 10 . ( a ) Kodi Satana anayesa bwanji kulepheletsa colinga ca Mulungu cokhudza mtundu wa Aisiraeli ? Komanso pamene Mfarisi anakhumudwa ndi zimene zinacitika , Yesu anakamba naye mokoma mtima . — Luka 7 : 36 - 48 . 14 Khalani Wokhulupilika kwa Yehova Iye anakauza atate wake za nkhaniyo . M’malo momusuliza , bwanji osaganizila zimene tingacite kuti tim’thandize kukula kuuzimu ? Pambuyo pake ife amoyo otsalafe , limodzi ndi iwowo , tidzatengedwa m’mitambo kukakumana ndi Ambuye m’mlengalenga , ndipo tizikakhala ndi Ambuye nthawi zonse . ” — 1 Ates . 12 : 14 ) Komabe , mogwilizana ndi zimene m’bale wa ku Thailand ameneyu anaona , nchito yakuthupi tifunika kuiona moyenela . Yaciŵili , kudzicepetsa kudzatithandiza kukhala ogonjela ndi oleza mtima pamene tiyembekezela kuti Yehova adzakonze zinthu zopanda cilungamo zimene zinacitika . Ngati alendo ocokela m’dziko lina ali kutali na kumene kuli Mboni zokamba citundu cawo , afunika kusonkhana na mpingo wa cinenelo ca m’delalo . ( Sal . Akulu a mumpingo wake anamuuza kuti aziwatumila foni ngati wabwelezanso kucita zimenezi . ( Aheberi 11 : 5 ) Kodi mtumwi Paulo anatanthauza ciani pamene anakamba kuti Inoki “ anasamutsidwa kuti asafe mozunzika ” ? 49 : 6 - 9 ) Koma Yesu anapeleka moyo wake wangwilo kaamba ka ife , ndi kupeleka mtengo wa dipo lake kwa Mulungu . ‘ Muiphele nsembe ya pasika . ’ ” — Eks . Eliya analibe maganizo akuti anthu akacita zinthu zoipa kapena zopanda cilungamo samalangidwa . ( 1 Tim . 4 : 10 ) Tiyeni tonse tipitilize kupita patsogolo pocita utumiki wopatulika kwa Yehova . Anthu akudya coimilila . ” AMBILI a ife tikamva mau akuti “ moyo weniweniwo , ” timaganizila za ciyembekezo ca moyo wosatha m’Paladaiso padziko lapansi . Muzifuna - funa Ufumu , Osati Zinthu Zakuthupi , July Kuganizila zimene zinacitikila Yesu atangobatizidwa kungatithandize kumvetsa kufunika kwa pempho lakuti : “ Musatilowetse m’mayeselo . ” Poonetsa kuyamikila , tiyeni tiziyesa - yesa kupewelatu macimo alionse amene anthu ena angawaone ngati ni aang’ono . Panthawiyo , n’nali na zaka 18 , ndipo n’nali kuyang’anizana ndi nkhani yongena usilikali . Mwina Mfumu Nebukadinezara anafuna kupangitsa Danieli kuganiza kuti Mulungu wake Yehova amalamulidwa na mulungu wa Ababulo . — Dan . Bukuli limafotokoza zimene Satana anakamba zakuti Yobu angakane Mulungu ngati angakumane na mavuto aakulu . Satana anapempha Mulungu kuti agwetsele Yobu masoka . Tikupemphani kudziŵa mphatso yaikulu imeneyi mwakuŵelenga nkhani yotsatila . Mwina Dema anayamba kukonda kwambili zinthu zakuthupi kuposa zinthu zakuuzimu . 7 : 9 , 13 - 15 . Titawapeza , io anatilandila ndi manja aŵili . 3 : 21 - 23 ; Aroma 1 : 20 ) Kapolo wokhulupilika amafalitsa mabuku ofotokoza Baibulo m’zinenelo zoposa 680 . Mtumwi Paulo anatilangiza ise Akhristu kuti tiyenela kupewa mzimu wosayamikila ufulu umene Yehova anatipatsa mokoma mtima kupitila mwa Mwana wake , Yesu Khristu . Nanga n’zinthu ziti zimene Satana sangakwanitse kucita ? Petulo ndi anzake ‘ anayendetsa ngalawazo ndi kufika nazo kumtunda , ndipo iwo anasiya ciliconse ndi kutsatila [ Yesu ] . ’ — Luka 5 : 1 - 11 . Ali wacitsikana , anali kukonda kwambili zandale . Ndipo sazengeleza kuphunzila njila zatsopano zolalikilila . Nkhaniyo inakambanso kuti kuwonjezela utumiki kumabweletsa cimwemwe coculuka . Pofika nthawi imene Yesu anafa , Yosefe ayenela kuti analibenso mantha ndipo anayamba kucilikiza ophunzila a Yesu . ( Ŵelengani Yoswa 1 : 8 . ) Cingafooke na kufa ngati siticilimbitsa . Iwo akafuna thandizo , tinali kuwathandiza mwa kuwaŵelengela zofalitsa zathu , ndi kupemphela nao pamodzi . ” “ Atate atangomwalila , mwamuna wanga anandiuza kuti wapeza mkazi wina . 24 : 20 ) Kodi Yehova anateteza bwanji anthu ake kwa adani amenewa kudzela mwa Yoswa , Mose , Aroni ndi Hura ? Komanso , ndise oyamikila ngako kuti Khristu anatibweletsa m’gulu la olambila oona amene ni ogwilizana . Tiyenela kukonda munthu aliyense , ndipo kucita zimenezi n’kofunika kwambili . Koma yesetsani kumuyandikila kwambili , ndipo iye “ adzakulimbitsani ndi kukupatsani mphamvu . ” ( 1 Pet . Kodi apeza madalitso otani cifukwa ca utumiki wao ? — Miy . Ndani Amadziŵa Zamtsogolo ? Ambili amaona kuti kunena munthu wa conco kuti adzalandila cilango m’helo , cabe cifukwa cakuti sanali Mkristu wobatizika , n’kupanda cikondi , ndipo n’kokhumudwitsa . TIMAKONDA Yehova “ cifukwa iye ndi amene anayamba kutikonda . ” Yesu ali padziko lapansi anaonetsa kulimba mtima m’njila zambili . 3 : 29 ) Conco , pangano latsopano limacilikiza pangano la Abulahamu . Ndiyeno pa mapeto pake , adzapeleka ufumu kwa Mulungu wake ndi Atate wake , atathetsa maboma onse , ulamulilo wonse , ndi mphamvu zonse . Tidzaphunzilanso zimene tingacite kuti tipitilizebe kuyang’ana kwa Yehova . Paulo anachulanso makhalidwe ena oipa amene amaonetsa kuti anthu alibe cikondi pa wina na mnzake . N’ciani coŵaŵa ngako kuposa ululu uliwonse umene tingamve cifukwa colandila cilango kapena uphungu ? N’cifukwa ciani Yesu anagwilitsila nchito fanizo la kanjele ka mpilu ? Gener , amene amakhala ku Asia , anakulila m’banja lacikristu , ndipo anabatizidwa ali ndi zaka 12 . Sukulu imeneyi inakambanso kuti , mwamuna angathetse cikwati ngati mkazi wanyetsa ndiyo kapena nsima kapena akaona mkazi wina wokongola kwambili . Paulo ? Onani Mateyo 6 : 11 , 34 . Timoteyo anasoŵa cokamba cifukwa ca udindo waukulu umene anapatsidwa . Tidzakhala na mtendele wa m’maganizo ndipo tidzakhalanso pamtendele na ena . Yehova watilemekeza kwambili mwa kutipatsa mwayi wocilikiza ulamulilo wake . Lomba nikamapemphela , nidzayamba kupemphela kwa Yehova . Yehova anayankha mafunso amenewo , ndipo anatitsimikizila zinthu ziŵili izi : ( 1 ) Iye afuna kuti mau ake alengezedwe “ pazilumba zakutali , ” ndi ( 2 ) afuna kuti anthu amene dziko limawaona kuti ndi otsika ndi onyozeka apeze citetezo m’dzina lake . — Yer . ( Eks . 6 : 12 ) Mose anauza Yehova nkhawa zake kuti apilile citonzo . Mpainiya akulalikila uthenga wofunika kwambili wa m’kabuku kakuti Uthenga Wabwino , kwa munthu amene akuyanika nyemba za koko Koma nthawi zonse anali kuuza ophunzila ake mmene anali kumvelela . Conco , anayamba kuonetsa kuwala kwawo mwa kulalikila panja pa nyumba yawo . Ndine m’bale wanu wokondedwa , Peter . ” Mneneli Yoweli ananena kuti nthawi imeneyo idzakhala “ tsiku lamdima ndi lacisoni . ” ( Yow . 2 : 1 , 2 ; Zef . Limodzi , aŵili , kapena onse atatu ? David : Gwen anandiuza zimene anali kuphunzila . 2 : 13 . Ndipo tinawakonda na mtima onse anyamata amene anasankha kuti amange nawo banja . Baibo inalembedwela anthu oona mtima amene amadalila thandizo la Mulungu kuti aimvetsetse . Buku la Chivumbulutso limayankha funso limeneli mwa kufotokoza za kuonongedwa kwa “ Babulo Wamkulu . ” 18 : 24 - 26 ) Makhalidwe amenewa ndi ofunika kwambili kwa ophunzila mofanana ndi manyowa m’nthaka , cifukwa amacititsa munthu kukula msanga mwakuuzimu . Cinthu cina cimene cimadetsa nkhawa anthu ambili ni ukalamba . Cifukwa cokunyuka kaŵilikaŵili , m’kupita kwa nthawi mafupa a Jairo anapindika . Kodi Ndalama Zoyendetsela Nchito Yathu Timazipeza Bwanji ? Kopotala wina dzina lake Ikumatsu Ota , anati : “ Tikangofika m’tauni , tinali kuimika kalavani yathu m’mbali mwa mtsinje kapena pamalo oonekela bwino . Muzidzifunsa mafunso pamene muŵelenga Baibo kapena mabuku ofotokoza Baibo . Mungadzifunse kuti , ‘ Kodi nkhaniyi iniphunzitsa ciani ponena za Yehova ? Monga Danieli , kodi winawake anakulimbikitsani kugwilitsila nchito luso lanu kuti mucilikize dziko la Satana ? ( 2 Akorinto 8 : 12 ) Koma palinso njila zina zimene tingaonetsele Yehova kuti timam’konda . Masiku amenewo , kukamba na Mboni za Yehova kunali koopsa . Koma zimene tinaphunzila kwa Apun zinasinthilatu umoyo wathu . 32 : 28 . Paulo anali nzika ya Roma , ndipo anafunika kuweluzidwa mwacilungamo . Wadela anatipempha kuti tisamukile ku Ruston , mu mzinda wa Louisiana kumene Mboni zambili zinali zozilala . Kodi anakumbukila mmene munthu ameneyu anavutitsila anthu a Mulungu kwa zaka zambili ? M’malo mwake tinafunika kulalikila m’dela la kutali limene abusa acipembedzo satidziŵa . Ngakhale zinali conco , iye anakumana ndi mavuto aakulu cifukwa ca zocita zake . Kuulula Macimo “ Ndinaulula chimo langa kwa inu , ndipo sindinabise colakwa canga . ” — Salimo 32 : 5 . Anali “ kukambilana lemba [ la tsiku ] m’maŵa uliwonse asanayambe kudya . Tsiku lililonse , apainiyawo anali kuyenda kukalalikila m’magawo awo osiyana - siyana mumzindawo . ” Poyankha funso limene Afarisi anafunsa Yesu , iye anati Mose analolela kuti anthu azisudzulana , “ koma kuyambila paciyambi sizinali conco ayi . ” ( Mat . Woyang’anila dela wina anafotokoza kuti iye ndi mkazi wake amagwilitsila nchito Baibulo kwambili . Kapena , kodi adzaona kuti ndi mwai kutengako mbali pa zocitika zimene zinaonekelatu kuti zinali kutsogoleledwa ndi Yehova ? ( b ) N’cifukwa ciani tifunika kudziŵa kuti n’zotheka kutaya cikhulupililo cathu ? Kodi munthu , kapena mbuye amaimila ndani ? Nanga talente imodzi inali yoculuka bwanji ? “ ZOKOLOLA n’zoculukadi , koma anchito ndi ocepa . Unasiya mkazi wako ali na pakati ndiponso mwana wako wamng’ono . Ponena za Mulungu , Baibulo limati : “ Nchito yake ndi yangwilo , Njila zake zonse ndi zolungama . Ngati mmodzi wa Mboni za Yehova amacita chimo , nthawi zambili mabwenzi ake amadziŵa . M’nkhani yoyamba tidzaphunzila mmene tingadziŵile kuti Mulungu amatikonda , ndiponso mmene tingaonele dzanja lake . Inde , ciliconse cimene timacita popititsa patsogolo zinthu za Ufumu wa Yehova zimaticititsa kukhala wolemela mwauzimu . Cifukwa cakuti anali wa luso pa nchito yake , anthu olemekezeka monga madokota na matica anali kusoketsa zovala kwa iye . Mwacitsanzo , ganizilani za Jumpei na mkazi wake , Nao , amene ali na zaka za m’ma 30 . ( b ) Kodi nkhani imene ili m’kabokosi yakuti , “ Pitilizani Kudziyesa . . . ” itiphunzitsa ciani ? Caka cimodzi ndi miyezi zinapita koma Cesar ndi Rocio anali asanaitanidwe ku Beteli . Kuti mudziŵe zambili zokhudza “ masiku otsiliza , ” onani nkhani 9 m’buku iyi , Zimene Baibulo Ingatiphunzitse , yofalitsidwa na Mboni za Yehova Pamene M’bale Harold King anali m’ndende , iye analemba ndakatulo ndi nyimbo zokhudza Cikumbutso Mofananamo , maganizo abwino amatithandiza kutsanzila Yehova . Koma , m’kupita kwa nthawi , ndinayamba kuwakhulupilila . Felisa : Pamene ndinayamba kutumikila Yehova , ang’ono anga anakhumudwa kwambili . 3 : 5 . Tsopano tiyeni tikambilane zozizwitsa zina zimene Yesu anacita ndi kuona mmene zimatikhudzila masiku ano ndi mmene zidzatikhudzila mtsogolo . Ndodo ziŵili zimene zinakhala ndodo imodzi ( Ezek . Kuti mumvetsetse cifukwa cake muyenela kuyamikila kwambili dipo , ganizilani izi : Tiyelekeze kuti muli m’madzi ndipo mwayamba kumila , kenako munthu wina wabwela kudzakupulumutsani . Olo kuti anali kudzifunsa mafunso amenewa , sanalole maganizo aconco kufooketsa cikhulupililo cake kapena kumulepheletsa kukhala wacimwemwe . Ndinamufunsa kuti ndidziŵe zimene zinamuthandiza kuŵelenga bwino motele atangoyeseza nthawi 30 cabe . Amakambanso kuti ngati tingakumane na mavuto , tingamusiye Mulungu . Mtundu wa Aisiraeli utayamba kulambila konama ndiponso kucita cinyengo ca kuuzimu , Mulungu anawacenjeza mobwelezabweleza za zotsatilapo zake . 4 : 14 ) M’malomwake , amayesetsa kuphunzitsa “ mphamvu zawo za kuzindikila ” kuti azikwanitsa “ kusiyanitsa coyenela ndi cosayenela . ” Patapita zaka zambili , Yehova anakhazikitsa cinthu cina capamwamba kupambana kacisi wakuthupi ameneyo . Tingatengele bwanji citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wacifundo ? Ganizilani cabe cisangalalo cimene ophunzilawo anakhala naco pamene Petulo anabwela na kuukitsa Dorika . Iye ni munthu woyamba wochulidwa m’Baibo amene anaukitsidwa na atumwi . ( Mac . Kodi tapatsidwa zida ziti zotithandiza kuseŵenzetsa luso la kulingalila ? Nditakwanitsa zaka 24 , amai anamwalila ndipo mkwiyo wanga unaonjezeka . ( Ezek . 37 : 24 , 25 ) Mgwilizano wocititsa cidwi umene unaloseledwa m’buku la Ezekieli , umaonekela kwambili pamene otsalila odzozedwa ndi a “ nkhosa zina ” asonkhana kuti akumbukile imfa ya Khristu caka ciliconse . Tiphunzilapo ciani pa zitsanzo zonsezi ? Izi zinandikhumudwitsa kwambili . Popeza mzimu woyela ni mphamvu yosaoneka , kodi Aisiraeli anadziŵa bwanji kuti unali kugwila nchito pa Mose ? Citsanzo cimodzi ni cimene cinafotokozedwa m’nkhani yakuti : “ Ndagwira Chovala cha Myuda kwa Zaka Zoposa 70 , ” imene ili mu Nsanja ya Olonda ya April 15 , 2012 peji 18 - 21 . Iye sanali kubala , koma mkazi mnzake , Penina , anali kubala . Ngati timaona kuti ndalama ndiponso katundu wathu n’zofunika kwambili , ndiye kuti zingakhale zovuta kupewa ndale . Anthu ena amaganiza kuti pemphelo limangokhazika mtima pansi . Njila yacitatu imene tingalimbitsile mgwilizano ni kukhululukila ena na mtima wonse . “ Maso a Yehova ali pa olungama . ” — 1 PET . Mu 2014 ndi mu 2015 , tinaseŵenzetsa masitediyamu akulu - akulu m’mizinda 14 padzikoli , pocita msonkhano wa maiko wa mutu wakuti , “ Pitilizani Kufunafuna Ufumu wa Mulungu Coyamba . ” ( Miy . 2 : 10 - 12 , 16 ) Zikakhala conco , dzifotokozeni kuti ndimwe wa Mboni za Yehova , muzicita zinthu mwaulemu , ndipo muzipewa kuceza mokopana cifukwa kumakhala na zotulukapo zoipa . Iwo adzamvela malangizo amene anapelekedwa m’nthawi ya Mfumu Yehosafati , akuti : “ Ulendo uno simufunikila kumenya nkhondo . “ Funsa , . . . zouluka zam’mlengalenga , ndipo zikuuza . Motelo , kutengela zocita za Yesu kudzatithandiza kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova , amene ndi wamkulu mu cilengedwe conse . Mfundo zothandiza pophunzila za pa jw.org zingakuthandizeni kucita zimenezi . Ndinali kudzicha kuti Msilamu . Atumiki a nthawi zonse amafunika kugwila nchito kuti azipeza zofunikila paumoyo . Makolo afunika kukhomeleza coonadi ca m’Baibulo m’mitima ya iwo eni . Cifukwa ciani ? Panali zinthu zambili zimene n’naona kuti siningakwanitse kucita , koma ndi thandizo la Yehova n’nazikwanitsa . ” Yehova anatilenga m’njila yakuti tizitha kugwila nchito mwakhama kuti tizisangalala ndi moyo . ( Mlal . 3 , 4 . ( a ) Kodi wolemba Salimo 71 anapempha ciani kwa Yehova mocokela pansi pamtima ? Cipatso ca mzimu umenewu cimaphatikizapo khalidwe la kudziletsa , limene n’logwilizana kwambili na kudzilanga tekha . Ngati ndinu okonzeka , mafunso amenewa sadzakucititsani kukaikila zikhulupililo zanu , koma adzakulimbikitsani kuphunzila Baibulo mwakhama . Mu 455 B.C E . , gulu la Ayuda , kuphatikizapo ana ambili , anasonkhana m’bwalo lalikulu mu mzinda wa Yelusalemu . Akulu a mumpingo umene anali kugwilizana nao anamuyamikila kaamba ka cikhulupililo cake ndi kulimba mtima kwake . Panthawiyo , Li mlongo wa zaka za m’ma 30 , anali kukhala m’dziko linalake ku Southeast Asia komweko . Nanga makolo angacite ciani kuti aseŵenzele pamodzi ndi Yehova pophunzitsa ana awo ? N’zoona kuti anthu ambili amapeleka mphatso na colinga cabwino . Kuyelekezela kwaconco kungacititse kuti kuŵelenga kwanu Baibo kukhale kothandiza kwambili . Ngakhale kuti anthu padziko lonse amavala zovala za masitaelo osiyanasiyana , ndipo mafashoni amasintha m’kupita kwa nthawi , mfundo za m’Baibulo sizisintha . Tikakhala opatsa , anthu enanso amalimbikitsidwa kukhala opatsa . Samuel anazindikila kuti kukopana si khalidwe loyela kapena loongoka . ( Ŵelengani Aefeso 1 : 9 , 10 . ) Yehova atawapulumutsa ku ukapolo ku Iguputo ndi kuwatsogolela m’Dziko Lolonjezedwa , iye anawalangiza mmene anayenela kucitila zinthu ndi anthu a m’dzikolo . 10 : 28 , 29 . Ndiponso pemphelo locokela pansi pa mtima linamuthandiza kupilila . Conco , mfundo zimenezi zikuonetsa kuti Akristu odzozedwa anali akapolo a Babulo Wamkulu kwa nthawi yaitali , osati cabe kucokela mu 1918 kufika mu 1919 . 6 Thanzi Labwino na Kupilila Msulami anali wokhulupilika kwa Yehova . — Nyimbo 2 : 1 , 2 ; 6 : 8 . Ndiyeno , anapatsa mnyamatayo zofalitsa zophunzilila Baibo , na kumulimbikitsa kuti aziphunzila Baibo na Mboni za Yehova . Tikakhala amtendele , ndiye kuti pakati pa olambila oona padzakhalanso mtendele woculuka . M’malo moganiza kuti , ‘ Ningacite ciani kuti niwine ? ’ M’maiko amenewo anthu lomba anali omasuka kukambilana nkhani za cipembedzo , ngakhale kutsutsa poyela ziphunzitso za machechi . Mwina anali kumwetulila kwambili ndipo nkhope yake inali kuoneka yowala ndi cimwemwe . Abale a ku Filipi ataŵelenga kalata imene Paulo anawalembela , anadziŵa kuti iye sanalembe maganizo ake . Paulo anapita m’mavuto aakulu . Panthawiyo , nchito yathu yolalikila inali yoletsedwa kumeneko . Koma tinavomelabe utumikiwo ngakhale kuti mkazi wanga zinam’dabwitsa poyamba . ( Yos . 23 : 2 , 14 ) Yehova analonjeza kuti adzapulumutsa anthu ake pa cisautso cacikulu ndi kuwapatsa moyo wosatha m’dziko latsopano . Abale akatifunsa mmene tinakumanilana , mwanthabwala timati , “ Ofesi ya nthambi ndi imene inakonza kuti tikumane . ” Pambuyo popezeka kangapo pa misonkhano , abale anatifunsa kuti , “ Kodi mufuna kubatizika ? ” Komabe , pali mafunso ambili amene asayansi sanapeze mayankho ake . Cozizwitsa cimeneci cikanaonetsa kuti Mose anatumidwadi ndi Mulungu ndi kuti iye anali naye . AFRICA : Mu 2013 , akuluakulu a m’boma pafupifupi 22,000 ku South Africa anawapeza ndi mlandu wocita ziphuphu . N’kuthekanso kuti tikuvutika cifukwa codziona ngati wosafunika , kugwilitsidwa mwala , kapena cifukwa ca zinthu zina zimene timalephela kucita bwino . Iwo anayankha kuti : “ Mwana wanga , n’cisinsi . 17 : 9 . Pangano la Abulahamu limatsimikizila kuti Ufumu wa kumwamba ndi weniweni , ndi kuti udzapeleka mwai kwa Mfumu ndi olamulila anzake kuti aloŵe Ufumuwo . ( Aheb . Kufuna kukhala payekha kapena na anthu ocepa . Pa November 11 , m’caka ca 1918 , Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse inatha . ( Mateyu 6 : 10 ) Zoonadi , panthawi yake yoikika , Mulungu , kudzela mu Ufumu wake , adzacotsa mavuto onse padziko lapansi . Iwo ayenela kutsatila uphungu wa oyang’anila acikristu wakuti : “ Wetani gulu la nkhosa za Mulungu lomwe analisiya m’manja mwanu , . . . Palibe buku lina limene lamasulidwa m’zinenelo zambili ngati Baibulo . N’cifukwa ciani tingakambe kuti kufeledwa mnzako wa m’cikwati n’kosiyana na ziyeso zina ? Komabe zimenezi sizitanthauza kuti tikapanga cosankha , sitiyenela kusintha zivute zitani . Ni pa zocitika ngati ziti pamene tifunika kuonetsa kuti timagwilizana ndi cilungamo ca Yehova ? Ngati ndinu mkulu , kodi zotele zinakucitikilamponi ? Iwo anabatizidwa m’caka cotsatilapo . Naonso atate anga a Ron , anaphunzila coonadi patapita zaka 13 . Solomo analemba kuti : “ Tumiza mkate wako pamadzi , cifukwa pakapita masiku ambili udzaupezanso . ” Timaonetsanso kuti ndife ogwilizana ndi abale ndi alongo athu padziko lonse pamene tipezeka pa Cikumbutso caka ciliconse . Onse ni okondwa ngako kumvela cilengezo capadela . Ulamulilo wake udzakhalapo mpaka kalekale ndipo sudzatha . Ufumu wake sudzaonongedwa . ” ( a ) Kodi Baibo ya Septuagint na ena akale anakhudza bwanji anthu amene anali kuŵelenga Mau a Mulungu ? Mosakaikila , mumafuna kuti Yehova alandile nsembe zanu zacitamando . Anacita zimenezi pamene analalikila kwa kazembe waciroma Koneliyo , pamodzi ndi acibale ndi mabwenzi ake . Nikalimbikitsa na kutsitsimula ena mwauzimu , inenso nimalimbikitsidwa na kutsitsimulidwa . ( Miy . 15 : 33 ) Mose anafunikila kuphunzila kuti akonzekele mavuto amtsogolo . ( Aef . 3 : 1 , 2 ) Paulo analamulidwa kulalikila uthenga wabwino kwa anthu amene si Ayuda . Zimenezi zinacititsa kuti anthu a mitundu ina akhale mbali ya boma lolamulidwa ndi Mesiya . Atate wathu walonjeza kuti adzatipatsa zonse zimene timafunikila . Mwacitsanzo , mwamuna wina ku Thailand atapezeka pa msonkhano wa cigawo , anacita cidwi kwambili na cikondi ca pakati pa abale na alongo . Koma sizinalandidwe mphatso ya ufulu wosankha zocita . Akhristu a m’nthawi ya Petulo anafunika kukhala ogwilizana pamene zinthu zinali kuipilaipila . Mwacitsanzo , ganizilani za mgwilizano wa mwamuna na mkazi m’banja . N’cifukwa ciani tiyenela kulemekeza nyumba za ena polalikila ? Don Adams N’cifukwa ciani nkhondoyi inasintha zinthu kwambili padzikoli ? ( Aefeso 6 :⁠ 1 ) Tengelani citsanzo ca Mulungu . ( Ezara 2 : 70 ) Anali na nchito yaikulu ngako . ( Ŵelengani Yesaya 55 : 6 , 7 . ) Mtundu udzaukilana ndi mtundu wina , ndipo ufumu udzaukilana ndi ufumu wina . . . Mau a Mulungu amatitsimikizila kuti macimo athu ‘ angafafanizidwe . ’ Panthawiyo , Kaisara anali wolamulila ndipo ndiye anali ndi udindo wapamwamba kwambili kuposa onse . 17 : 3 ) Kuti mukhomeleze mfundo zimenezi mwa iwo mukhoza kusankha cocitika kapena cokumana naco m’zofalitsa zathu . Mwacitsanzo , kumbukilani nkhani ya mahule aŵili amene anali kulimbilana mwana pamaso pa Solomo . Ngakhale kuti mwina takhala tikulimbana na mavuto amodzi - modzi kwa nthawi yaitali , “ tisaleke kucita zabwino , pakuti pa nyengo yake tidzakolola tikapanda kutopa . ” ( Agal . Ni “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” cabe amene Yehova anamupatsa udindo wopeleka cakudya cauzimu . ( Mat . N’cifukwa ciani a “ nkhosa zina ” naonso angapindule ndi fanizo la anamwali 10 ? Mkambi anafotokoza zimene anthu amene akufuna kuonjezela utumiki wao angacite . Inafotokozanso kuti “ abale ” a Mfumu ndi anthu amene adzalamulila ndi Yesu kumwamba , ndiponso onse amene adzakhala ndi moyo padziko lapansi akadzakhala angwilo . Anati : “ Mudzadziŵa coonadi , ndipo coonadi cidzakumasulani . ” ( Yoh . Mwacidule tingakambe kuti : Mulungu amasankha nthaŵi imene angaonetse mphamvu yake yodziŵilatu zamtsogolo malinga ndi mmene afunila . 9 , 10 . ( a ) N’cifukwa ciani Ayuda sanali kufunika kunyadila mtundu wawo ? Kodi muli na anzanu a makhalidwe otani ? Nthawi zambili timakambilana ndi anthu panyumba zao . N’cifukwa ciani kamvedwe kathu katsopano kameneka n’koyenelela ndiponso kolondola ? Ndinaganiza kuti , ‘ pokhala wacicepele , cinali cinthu cacing’ono kwa Mulungu kukwanilitsa zimene mtima wanga unali kufuna . ’ Conco , mwamuna afunika kuganizila zimene angacite kuti mkazi wake azim’lemekeza nthawi zonse . Ngati wodwalayo ali pafupi kumwalila , kodi mungacite ciani ? Ndinadabwa kuona kuti poŵelenga sanali kugwila pa Baibulo lake monga mmene anali kucitila poyamba . 145 : 10 - 12 ) Mau amenewa aonetsa mmene atumiki onse a Yehova okhulupilika amamvelela . Pamene n’naikidwa kukhala woyang’anila cigawo , n’nafunikanso kupanga masinthidwe ena . Apa Paulo anali kunena za kuthandiza acibale amene ndi Akristu , koma makolo amene si Akristu naonso sayenela kunyalanyazidwa . Satana angasokoneze motani maganizo a anthu ? Karen ( pakati ) Ine ndi mwamuna wanga tifuna kuti tilele mwana wathu m’malangizo a Yehova . Mungaonenso Mateyu 26 : 39 ; ndi 1 Akorinto 15 : 28 . Cifukwa cimodzi n’cakuti nthawi zina Yehova sayankha mapemphelo pa nthawi yomweyo . — Sal . 24 : 21 ; Chiv . 12 : 12 ) Conco , tiyenela kuyembekezela kuti zinthu padzikoli zidzaipa kwambili mtsogolo kuposa masiku ano . Koma anthu ena anasuliza zimenezi , ndipo anakamba kuti mavesiwa apangitsa Baibulo kukhala m’zidutswazidutswa . N’kutheka kuti makolowo sanali kuyembekezela zimenezi , koma angalandilebe mphatsoyo cifukwa ni njila imene mwanayo angaonetsele kuti amayamikila zimene makolowo amam’citila . Yesu anaphunzitsa anthu zinthu zofunika kwambili ndiponso zozama , koma anagwilitsila nchito mau osavuta kumva . Tiyeni tiyesetse kutsatila citsanzo cao ca kudzicepetsa ndi kutumikila Mulungu modzipeleka . Ena amakonda kuŵelenga Baibulo m’maŵa ndi m’madzulo asanapite kukagona . Ngati tikuvutika kuthetsa cilakolako coipa , n’cifukwa ciani tifunika kupempha thandizo ? Kumbukilani kuti Yesu anauza ophunzila ake kuti panali zinthu zina zimene iwo sanali kuzidziŵa ndipo sakanazidziŵa . 10 : 24 ) A Samuel , amene ndi atate ake Joshua ndi Esther , anati : “ Ine na mkazi wanga tinali kuona mmene ana athu anali kucitila mwauzimu kuti tidziŵe citundu cimene cingawathandize kupita patsogolo . Sin’nali kudziŵa kuti m’zaka za kutsogolo , nidzakhala na mwayi wokacezela abale m’maiko amenewo . ( b ) Kodi kuonetsa mzimu wa ubwenzi kuli na ubwino wanji ? ( Luka 2 : 36 , 37 ) Mukamapezeka pa misonkhano ndi kutengamo mbali mmene mungathele , mumadzilimbitsa ndiponso mumalimbikitsa ena . 15 : 53 ) Kaya tili ndi ciyembekezo ca moyo wa kumwamba kapena padziko lapansi , panthawiyo sitidzakumana ndi mavuto amene alipo masiku ano . Malemba amatiuza tanthauzo la salimo imeneyi . Monga mmene zinalili kwa Yesu ndi makolo ake , anthu othaŵa kwawo sangafune kubwelela kudziko lawo ngati amene anali kuwazunza akali kulamulila . Sitingakambe motsimikiza . Koma kodi Mulungu anam’siya Yosefe ? Pali umboni wanji wotsimikizila kuti m’tsogolo kudzakhala ciukililo ? Anaiponya pansi ndipo inasanduka njoka . Pamenepo Mose anayamba kuthaŵa . Mwa kucita izi , mudzayala maziko abwino othandizila mwana wanu kudziŵa kuti kudzipeleka na kukhala Mkhristu ni nkhani yaikulu , ndiponso kumabweletsa madalitso oculuka . Koma kodi anakhumudwa podziŵa kuti ndi anthu ocepa amene anaona nchito yao ? 7 : 28 ) Kodi cofunikila n’ciani kuti nsautso imeneyo izicepako ? Patapita nthawi , Davide anatumiza anyamata ake kwa Nabala kuti akapempheko cakudya ‘ ciliconse cimene dzanja lake [ la Nabala ] linapeza . ’ ( 1 Sam . Thomas , m’bale amene ali na mwana wa zaka 11 anati : “ Nthawi zina , mwana wanga amafunsa mafunso monga akuti , ‘ Kodi n’kutheka kuti Yehova anaseŵenzetsa cisanduliko polenga zamoyo padziko ? ’ Koma kodi kucita zimenezi kungathandize mwana wawo kukhaladi na umoyo wopambana ? ( Chalichi cimamasulila molakwika mau a Yesu a pa Mateyu 16 : 18 , 19 . ) Pochula zocitika za m’nthawi ya Mose , Paulo anali kukumbutsa Timoteyo kufunika kocitapo kanthu kuti ateteze ubwenzi wake wamtengo wapatali ndi Yehova . Abale ake ambili a Lije anakhala zaka zambili m’makampu a United Nations a anthu othaŵa kwawo . ( Yoh . 6 : 68 , 69 ) N’ciani cinawathandiza kutsimikiza kuti Yehova anali kutsogolela anthu ake kupitila mwa Yesu Khiristu ? Koma n’nangoona kuti nasiliza kugaŵila tumabuku tonse . Nthawi iliyonse pokacititsa phunzilo , n’nali kuyesetsa kukonzekela bwino . Koma tanthauzo la loto la mkulu wa ophika mkateyo silinali labwino . Ndi zifukwa ziti za m’Malemba zocotsela munthu mumpingo ? ( Deut . 34 : 10 ) Olo kuti Mose anali pa ubwenzi wolimba na Yehova , iye anataya mwayi woloŵa m’Dziko Lolonjezedwa . ( Num . Asayansi sanali kudziŵa zeni - zeni pankhaniyi . Anadziŵa izi pambuyo pa zaka zambili . — Yobu 26 : 7 ; Yesaya 40 : 22 . Pamene Nowa anamanga cingalawa , anaonetsa kuti anali na cikhulupililo . Masiku ano , tuakacisi tungakhale malo opatulika , chalichi , kapena malo ena ake amene munthu amalambilila . Mwacitsanzo , Robert anati : “ Ine ndi mkazi wanga tinali ndi zaka pafupi - fupi 55 pamene tinaona kuti tili ndi mipata yambili yotumikila Yehova . ( b ) N’ciani cingaticitikile ngati tinyalanyaza macenjezo ? NYIMBO : 89 , 140 13 : 13 ) Cimatidziŵikitsa kuti ndise otsatila a Yesu . Davide anati : “ Ndani angakwele m’phili la Yehova ? Ndipo ndani anganyamuke kukaloŵa m’malo ake opatulika ? Ndiye cifukwa cake Baibulo limakamba kuti munthu woyamba ndi “ mwana wa Mulungu . ” Tisaiŵale kuti atumiki anthawi zonse ndi otangwanika kwambili ndi nchito yolalikila , imene ndi yofunika kwambili padziko lonse masiku ano . ( Mat . Mlongo Ute watumikila ku Madagascar kwa zaka pafupifupi 23 . Mau okopa a mkaziyo anadzutsa cilakolako coipa mwa mnyamatayo ndipo analephela kudziletsa . Acicepele ambili amatangwanika na mafoni awo , mamotoka , nchito , na zinthu zina . Monga mmene tafotokozela , Olipa ‘ anabwelela kwa anthu a kwao ndi kwa milungu yake . ’ Kudzoleka gilisilini pa milomo ya wodwala , na kuika pa mphumi pake kathaulo konyowa zingathandize kuti amveleko bwino . Tsopano m’maiko amene anali mbali ya Soviet Union muli ofalitsa oposa 400,000 ! Poyankha pemphelo la Asa locokela pansi pa mtima , Mulungu anamuthandiza kugonjetsa kothelatu gulu lankhondo la Aitiyopiya . Koma Kristu anaukitsidwa , ndipo zimenezi zinatsimikizila kuti zimene anaphunzitsa ndi zimene anakamba ponena za mtsogolo n’zoona . — Ŵelengani 1 Akorinto 15 : 14 , 15 , 20 . Wokwelapo wake dzina lake anali Imfa . Yankho lililonse limene mwininyumba angapeleke pa mayankho atatuwo , tembenukilani patsamba la mkati ndi kukamba kuti , “ Baibulo limanena kuti ‘ Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu . ’ ” Michael anadzimvela cisoni atazindikila kuti wakamba zinthu mosaganizila mnzake ndi mopanda cikondi . Kodi Yesu anacita bwanji na khalidwe limeneli ? Acicepele ambili amayesetsa kusakila nchito , koma sazipeza . Mudzasangalala kudziŵa zina mwa zida ndi njila zatsopano zimene timagwilitsila nchito polalikila . Kodi Jumpei ndi Nao amapeza bwanji zofunikila mu umoyo wawo ? M’zaka za pakati pa 500 C.E . ndi 1500 C.E . , anthu okonda Baibulo anapitiliza kuimasulila ndi kukopela Malemba ake ngakhale kuti anali kuzunzidwa kwambili . kuthandizidwa ndi angelo ? 12 Kodi Maso Anu Amayang’ana kwa Ndani ? Ndinacita cidwi kudziŵa kuti ziphunzitso zambili monga Utatu ndi kuti mzimu wa munthu sukufa , n’zosagwilizana ndi Malemba . ( Mlal . 9 : 5 , 10 ; Yoh . Luis , amene tamuchula m’nkhani yoyamba , ali na vuto lalikulu la mtima , ndipo maulendo aŵili anatsala pang’ono kufa . Tingapambane bwanji pankhondo yolimbana ndi zilakolako zathupi ? Kukamba zoona , maphunzilo a ku Giliyadi ananithandiza kukula mwauzimu . Lemba la 1 Petulo 1 : 8 , 9 linalembedwela Akristu amene ali ndi ciyembekezo cakumwamba . Anthu amakhulupilila kuti zinthu zimenezi zimatsogolela umoyo wa anthu padziko lapansi . Fotokozani cifukwa cake ziyenela kuti zinali zovuta kuti Mose akwanilitse utumiki wake . ( Salimo 16 : 7 ) Davide anasinkhasinkha malangizo a Yehova ndi kuwamvela ndipo anasintha maganizo ake ngakhale kuti sicinali copepuka kutelo . M’kupita kwa nthawi , anthu a Yehova anayamba kufalitsa uthenga wa Ufumu padzilo lonse kupitila pa wailesi . Makolo angapeze malangizo othandiza m’buku lakuti Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa , Buku Loyamba , tsamba 317 , ndi Buku Laciŵili , tsamba 136 mpaka 141 . Lonjezo la Yefita linali losiyana ndi la Hana . Kubuula capansi pansi kungacitike cifukwa cakuti mitsempha ya pa khosi sikuseŵenza bwino . Malemba amatitsimikizila kuti “ Yesu Khristu ali cimodzimodzi dzulo ndi lelo , ndiponso mpaka muyaya . ” Munthu wina woimila kampani yochedwa , Decca Record Company , amene anakana kujambula nyimbo za gulu loimba lochedwa Beatles mu 1962 , anali kukhulupilila kuti magulu oimba magita adzatha m’tsogolo . Khalani oleza mtima . TSIKU limene Yesu anaukitsidwa , ophunzila ake aŵili anali kupita ku mudzi wina umene unali pamtunda wa makilomitala 11.2 kucokela ku Yerusalemu . 16 , 17 . ( a ) N’ciani cimene anthu a Mulungu anali kufunikila ? Iye anaziyelekezela ndi mfumu ndi wansembe pa zifukwa zosadziŵika bwino . Mofananamo , makolo ayenela kulanga ana ao mosamala ndi mwacikondi . Maulamulilo andale amene akuimilidwa ndi “ nyanga 10 ” sadzaloledwa kuononga anthu a Mulungu . Kodi mungawapemphe kuti mupite nawo mu ulaliki ? Kodi Yehova wapeleka ziyembekezo ziŵili ziti ? Mwacitsanzo , iye anawauza kuti ayenela kukhala okoma mtima . Anawauzanso kuti ayenela kukhala mwamtendele ndi ena , kuthetsa mkwiyo , kuthetsa mikangano mwamsanga , ndi kukonda adani ao . — Mateyu 5 : 5 , 9 , 22 , 25 , 44 . Kuti munthu ayenelele ubatizo , kodi ayenela kudziŵa zonse ? Ufumu wa Mesiya ndiwo makonzedwe a Wamphamvuyonse amene adzakwanilitsa cifunilo cake ponena za cilengedwe . Cilamulo cinakwanilitsidwa pamene Kristu anabwela padziko lapansi . Ngati anacokela kumadela a kumidzi , sangadziŵe moseŵenzetsela zipangizo zamakono zam’nyumba . Tikalibe kuloŵa m’dziko latsopano . Nkhani imeneyi imatikumbutsa za kukhulupilika kwa Kristu ndi odzozedwa . ( a ) Kodi masomphenya a namba 8 a Zekariya anayamba bwanji ? 15 : 8 ) Conco , ngati timaganizila mozama pemphelo lacitsanzo , tingazindikile zinthu zofunika kwambili zimene nthawi zina timazinyalanyaza . Ngati ndimwe wodzicepetsa , mumakhala ngati mwatsegula “ njila ” na kuilambulila kuti anthu akhale omasuka kupempha cikhululukilo kwa inu . Nepal 3 : 13 ) Malinga ndi mau a Paulo , panthawi ino tidzakumanabe ndi masautso . Anati : “ Ndidzamudalitsa ndipo iwe ndidzakupatsa mwana wamwamuna wocokela mwa iye . Ndidzamudalitsa ndipo adzakhala mayi wa mitundu yambili ya anthu ndi wa mafumu a mitundu yambili ya anthu . ” — Genesis 17 : 5 , 15 , 16 . 32 : 10 ; Luka 5 : 8 ) Nanga akanacita “ mantha ” monga mmene ophunzila a Yesu anacitila ? Kapena kodi angelo olungama akanafunika ‘ kulimba mtima ’ polalikila uthenga wabwino uku akutsutsidwa monga mmene Paulo ndi ena anacitila ? Kumvela Cenjezo Kumapulumutsa 11 Munthu safunika kucita kumangika kapena kuyang’ana kumbali cifukwa ca mmene tavalila . Cifukwa cakuti munthu wina anawanamizila kuti anacita zinthu mwacinyengo . Anthu amakamba zimenezi cifukwa cakuti alibe cikhulupililo . 15 : 21 - 28 . Baibulo limati : “ Njila ya olungama ili ngati kuwala kwamphamvu kumene kumamka kuonjezeleka mpaka tsiku litakhazikika . ” ( Miy . Apa m’pamene anali kufunika kutsatila kwambili mfundo ina ya m’Cilamulo ca Mulungu imene imati : “ Musamaweluze mopanda cilungamo . TSAMBA 24 • NYIMBO : 12 , 69 Pamene muŵelenga , mungaime pang’ono na kuyamba kusinkha - sinkha . Mkhristu aliyense ali na ufulu wosankha zosangulutsa zimene wakonda , ndipo mitu ya mabanja nayonso ingasankhile banja lawo zosangulutsa . Komabe , zosankhazo zifunika kukhala zogwilizana ndi mfundo za Yehova zopezeka m’Baibo . Baibo ingakuthandizeni kupeza citonthozo ngakhale pa nthawi zovuta kwambili Patsiku ndinali kukoka ndudu 20 za camba , ndinalinso kuseŵenzetsa mankhwala a mtundu wa heroin ndi mitundu ina yoletsedwa . Dipo inacititsa kuti zikhale zotheka kusonkhanitsa a 144,000 kuti akatumikile monga mafumu ndi ansembe pamodzi na Khiristu kumwamba . Timamva za zocitika za anthu amene anapempha thandizo kwa Mulungu ndipo iye anayankha mapemphelo ao . Ineyo ndikuthandiza . ” Koma kodi kucita zimenezi kuli ndi vuto lotani ? Koma iye anati Mulungu “ anangokhala cete . ” Akulu angakonze zakuti pakhale nkhani ya zosoŵa za pampingo pa Msonkhano wa Nchito pogwilitsila nchito nkhani imene inatulukapo malinga ndi zosoŵa za pamalopo . Angapelekenso cilengezo cokhudza nkhaniyo mwa njila yosakhumudwitsa ena . Musayese kumuganizila mwa njila imeneyi . Onani ndime 17 . Mlongo wina , dzina lake Kayla , ali na matenda amene amam’cititsa kuti azikhala wotopa nthawi zonse . Yesu anapatsa malangizo ofanana ndi amenewa ku “ kagulu ka nkhosa ” ka otsatila ake odzozedwa . Iye anati : “ Mangani m’ciuno mwanu ndipo nyale zanu zikhale ciyakile . Inuyo mukhale ngati anthu amene akuyembekezela kubwela kwa mbuye wao kucokela ku ukwati . ” N’zosangalatsa kuona kuti Jairo mothandizidwa ndi m’nzake wa Mboni , pang’onopang’ono anaphunzitsa Baibulo ambuya . Uyo akubwela apoyo . Yehova amachula Akhiristu odzozedwa olungama kuti ana ake , ndipo a “ nkhosa zina ” olungama kuti mabwenzi ake . ( Yoh . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti kuimba nyimbo n’kofunika pa kulambila kwacikhristu ? Ngakhale zinali conco , iwo anali na makhalidwe oipa ndipo sanali paubwenzi wabwino na Mulungu . Mosiyana ndi wokwela pa hosi yoyamba , amene akuimila munthu weni - weni , mahosi atatu otsatila akuimila zocitika zimene zikhudza anthu ambili padziko lonse . “ Pamenepo , hachi ina inatulukila . 6 : 33 , 34 ) Patapita nthawi , bwana wake wakale anamuitana ndi kumupempha kuti ayambenso kugwila nchito imene anali kugwila poyamba . Zotsatilapo za nchito yolalikila kaŵilikaŵili zimaonekela pambuyo pa zaka zambili nchitoyo itagwilidwa . Pakali pano , zimene tidziŵa n’zakuti Mau a Mulungu amanena kuti imfa ndiyo mapeto a cikwati . ( Maliko 10 : 29 , 30 ) Izi n’zimene adzayang’anizana nazo pambuyo pobatizika . Nthawi zambili onse m’banja angafune kuti makolo okalamba azikhala okha . M’malo mwake , tiyenela kukhala “ mtundu wa anthu okhala ndi cikhulupililo . ” ( Yoh . 10 : 16 ) Monga mmene Yesu anafotokozela , anthu onse a Mulungu masiku ano ndi ogwilizana kaya ali ndi ciyembekezo cokakhala kumwamba kapena padziko lapansi . Pamene Jairo anapitiliza kulimvetsa Baibulo , anayamba kufunitsitsa kuthandiza ena mwakuuzimu . Ndipo adziyankha kuti , ‘ Ndimafuna kuti azichaya nane bola . ’ Iye analemba kuti : “ A Mboni inu mwanicititsa cidwi kwambili . Ganizilani malangizo a pa Afilipi 2 : 3 , 4 , akuti : “ Musacite ciliconse ndi mtima wokonda mikangano kapena wodzikuza , koma modzicepetsa , ndi kuona ena kukhala okuposani . Musamaganizile zofuna zanu zokha , koma muziganizilanso zofuna za ena . ” Pelekani citsanzo coonetsa mmene zocita zathu mu ulaliki zingakhudzile ena . Koma pamene Hana anali kuganizila mmene zidzakhalila akadzapeleka mwana wake Samueli ku Cihema , sanali kuganizila zinthu zosatheka . Mairambubu ananiuza kuti , “ Namva zinthu zokondweletsa kwambili . Yesu anakamba kuti kukhala wosakwatila inali “ mphatso ” imene si otsatila ake onse anali nayo . M’bale Russell sanafune kuti anthu azim’tamanda . Musaiŵale zimene Yesu anali kukamba pochula mfundo imeneyi . ( Yak . 1 : 22 - 25 ) Nduna ya ku Itiyopiya ya m’nthawi ya atumwi inamvetsetsa mfundo imeneyi . “ Mulole kuti kupilila kumalize kugwila nchito yake , kuti mukhale okwanila ndi opanda cilema m’mbali zonse , osapelewela kalikonse . ” — YAKOBO 1 : 4 . Yesu sanali kukamba za msodzi mmodzi amene amagwilitsila nchito mbedza ndi nyambo kuti akole nsomba . Anthu abwino adzakhala na mtendele woculuka padziko lapansi kwamuyaya . — Salimo 37 : 9 - 11 , 29 . Mkhristu angayambe cibwenzi ndi munthu amene sakonda Yehova , cifukwa coganiza kuti pakati pa Akhristu palibe munthu womuyenelela . Pamene anali wacicepele , Luther anaona kuti Lefèvre anamasulila nkhani za m’Baibo m’njila yolongosoka ndi yosavuta kumvetsetsa , kusiyana ndi mmene akatswili ena a Baibo a m’nthawi yake anacitila . Nanga anamva bwanji pamene anaona munthuyo amene anali wa maonekedwe oipa ? Kodi tingaganize kuti cifukwa cakuti palibe ciliconse cacitika ndiye kuti Yehova sanatiyankhe ? Mukamapemphela , muzipempha kuti Yehova athandize ana anu ndiponso kuti akuthandizeni inuyo panokha . ( Mika 6 : 8 ) Kusadalila kwambili nzelu zanu kapena maluso anu , kudzakuthandizani kucepetsako nkhawa cifukwa mudzayamba kudalila Mulungu . Nthawi ina , Yesu atacoka ku Isiraeli kupita m’dela la Siriya m’dziko la Roma , mayi wacigiriki anapita kwa iye kukapempha thandizo . Ndithudi ! Atumiki a Mulungu akuonetsa kuwala kwawo . Pelekani citsanzo . Monga nyumba imene nthawi zina imang’ambika , kusemphana maganizo kuli monga ming’alu ing’onoing’ono imene ingawononge mgwilizano wathu . Ngakhale kuti tili na umoyo wosalila zambili , tili na zonse zimene zingatithandize kukhala osangalala . Simufunikila kupeleka ndalama kuti mukapezeke pa cocitika cimeneci . Koma kholo limene limakondadi mwana wake , limakana kum’patsa ngati zimene akufunazo n’zosafunikila . Anthu anafunika kusamba pambuyo pogwila mtembo . Palibe njila ina yosonyezela cifundo anthu amene afuna kuphunzila Baibulo kuposa kuwalikila . 19 : 3 - 6 ) Kodi iwo anasankha ciani ? Kodi Yehova wawadalitsa cifukwa ca kudzipeleka kwao ? Masiku ano , Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova limapeleka cilimbikitso kwa atumiki a pa Beteli , atumiki ena a nthawi zonse apadela , na ku gulu lonse la abale padziko lapansi . Makolo a Maria anasangalala kwambili pamene mwana wawo anasankha kudzipeleka kwa Yehova na kubatizika . Nafenso timafuna cilimbikitso m’nthawi yovuta ino . — Aroma 1 : 11 , 12 . M’bale Mumba : N’zoona zimenezo . ( Ŵelengani Danieli 12 : 3 . ) Conco , Mulungu woona anasintha maganizo ake pa tsoka limene ananena kuti awabweletsela , moti sanawabweletsele . ” Mau ake amatiuza za iye ndiponso mmene amacitila zinthu ndi anthu . Buku ina ya mbili yamakono yakuti Mapping Paradise , ili ndi nkhani zokhudza mamapu akale oposa 190 . Ambili amaonetsa mapikica a Adamu ndi Hava m’munda wa Edeni . Zikakhala conco , okwatilanawo ayenela kuzindikila kuti afunika kuuzana mau acikondi cifukwa zimenezi zidzathandiza kuti cikondi cao cilimbe , ndipo cikwati cao cidzakhala copambana . ( 1 Akor . 2 : 14 ) Mosiyana ndi anthu a m’dzikoli , ife tili ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha ndi kudzaona anthu akufa aukitsidwa . Nanga n’cifukwa ciani umayang’ana kacitsotso m’diso la m’bale wako , koma osaganizila mtanda wa denga la nyumba umene uli m’diso lako ? Mosakaikila , nayenso Yehova Mulungu amamuyewa mkazi wokhulupilika ameneyu , ndipo alaka - laka kudzamuukitsa m’paradaiso padziko lapansi . Amafunitsitsa kukhala na mwana , koma alibe mphatso yobala . Usiku uliwonse , n’nali kuona ndeke za ku Germany zoponya mabomba zikuzungulila dela lathu . Atate amacititsa Kulambila kwa Pabanja mlungu uliwonse . ( Luka 5 : 27 , 28 ) Inenso nakhala na mwayi wocita zofanana na zimenezi . Kumvetsetsa mfundozo kumaphatikizapo kudziŵa bwino maganizo a Mulungu , amene ndiye Wopeleka malamulo , komanso kumvetsetsa zifukwa zimene anapelekela malamulowo . Koma kuti tiyanjidwe na Mulungu , cinthu cofunika ngako ni kucilikiza kulambila koona mosalekeza . Munthu amene amaŵelenga Mau a Mulungu nthawi zonse , amakhala “ ngati mtengo wobzalidwa m’mphepete mwa mitsinje ya madzi , umene umabala zipatso m’nyengo yake , umenenso masamba ake safota , ndipo zocita zake zonse zidzamuyendela bwino . ” — Sal . Tonse timamvela bwino kukhala paubwenzi ndi banja lathu ndi anzathu amene amatikonda , amatiyamikila , ndi kutidziŵa bwino . Zikakhala conco simuyenela kukwiya . Mu 1943 , n’nabatizika mu mzinda wa Blackpool , ku England . Koma tsopano timacita ndipo ndi dalitso . ” N’ciani cimakucititsani cidwi mukaganizila cifukwa cake Yesu anali kucita zozizwitsa ? Lomba tiyeni tikambilane zinthu zitatu zimene zingatilepheletse kukhala maso . Mlongo wina ku Australia anakhudzika mtima ataŵelenga nkhani yofotokoza tanthauzo la Pasika mu Nsanja ya Mlonda ya December 15 , 2013 . Petulo anacita kulengeza poyela kuti sadzasiya Mbuye wake , koma tsiku limenelo usiku , anakana Yesu kuti samudziŵa . — Mat . ( Miy . 4 : 23 ) Msilikali sangasinthanitse codzitetezela pacifuwa copangiwa na citsulo colimba n’kutenga cina copangiwa na citsulo cosalimba . Na ise n’cimodzi - modzi . Ambili mwa Ayuda amenewo anali kutengela nzelu za Yudasi Mgalileya . Koma timakhulupilila kuti Yehova ni amene akutsogolela mpingo ndipo nthawi zonse amacita zinthu zoyenela . Zimene Paulo anacita pa milandu yabodza zikutiphunzitsa mfundo zofunika . Kusinkhasinkha za Yehova ndi Yesu kungathandize Mkristu kukhala wokhwima kuuzimu ndi kukhalabe ndi cikhulupililo colimba . N’zacisoni kuti m’malo mosankha kumvela lamulo la Mulungu kuti akhale na moyo kwamuyaya , Adamu anasankha kusamvela . Eyaa , ndi apa pamene tifuna . Paulo anauza Akristu odzozedwa kuti : “ Ine , amene ndili m’ndende cifukwa ca Ambuye , ndikukucondelelani kuti muziyenda moyenela kuitana kumene munaitanidwa nako . ” “ Pakuti Yehova wanena kuti : . . . Cifukwa copandukila Mulungu , Adamu ndi Hava anakhala opanda ungwilo . Komanso , banja limene lingaoneke lolimba likhoza kuonongedwa ndi “ nchito za thupi , ” monga dama , khalidwe lotayilila , udani , ndeu , nsanje , kupsa mtima , ndi mikangano . — Agal . Alongo athu amene akutumikila kumalo osoŵa ku maiko acilendo amati kutumikila m’maiko ena kwawapatsa madalitso ambili . 3 “ Ufumu Wanga Suli Mbali ya Dziko Lino ” “ Bwelelani kwa ine , . . . ndipo ine ndidzabwelela kwa inu . ” — ZEK . Kodi zocita za mabungwe acinyengo zimatikhudza bwanji masiku ano ? ( Genesis 9 : 4 ; Machitidwe 15 : 28 , 29 ) Tingapemphe Yehova kuti atithandize kupanga zosankha zimene zidzam’kondweletsa . 16 : 17 ; Aheb . 4 : 13 ) Yehova amatiyang’ana cifukwa amatikonda ndipo amafuna kuti tikhale otetezeka ndi acimwemwe . — 1 Pet . Ndipo sikulakwa kuika cipilala pa manda a munthu amene anafa . ( Sal . 116 : 12 ) Kodi mukanayankha bwanji ngati munthu wina akanakufunsani kuti , ‘ Ndi zinthu ziti zimene Yehova anakucitilani zimene mumayamikila ? ’ Pa tsiku limenelo padzakhala anthu ophedwa ndi Yehova kucokela kumalekezelo a dziko lapansi kufikanso kumalekezelo ena a dziko lapansi . 54 : 7 , 8 . Mzimu umenewu ndi wofala kwambili . N’ciani cingathandize munthu kuvula umunthu wakale ? M’nkhani yotsatila , tidzakambilana zinthu zina zamakono zimene zatithandiza kufalitsa uthenga wa Ufumu kwa anthu a mitima yabwino padziko lonse lapansi . Koma n’nali wofunitsitsa kukhala monga Yesaya , amene anati : ‘ Ine ndilipo ! Amayi anali Mkatolika wokangalika , ndipo anali kufuna kuti ine nikakhale sisitele . Pambuyo pa Aramagedo , tidzaona pamene panali kukhala oipa , koma sadzapezekapo . Cesar anati : “ Tinasandutsa galaji yathu kukhala nyumba ya cipinda cimodzi n’colinga cakuti tizicititsa lendi nyumba yathu . ( Mac . 8 : 32 - 38 ) Mofananamo , mabuku athu ofotokoza Baibulo amatithandiza kudziŵa coonadi molondola . Iye amafuna kuti io adzakhale ndi moyo wabwino . NYIMBO : 142 , 12 Komabe , timatsimikiza kuti Mulungu amadziŵa kuti ndife fumbi , ndi kuti ni wofunitsitsa kuticitila cifundo . ( Sal . Yehova anadalitsa Sara cifukwa ca cikhulupililo cake N’ciani cingatithandize kupilila ? MABUKUWO anali kuchedwa mpukutu wa utawaleza . Panthawi yake , ulamulilo wa Mulungu udzadziŵika kuti ndiwo woyenela , koma ulamulilo wa Satana ndi anthu udzalephela ndipo udzathetsedwa . Tsiku lina n’nakolewa kwambili cakuti n’tadzuka m’maŵa , sin’nathe kukumbukila mmene n’nafikila panyumba . ( Miy . 12 : 18 ) Pofuna kutonthoza ena , ambili apeza mfundo zolimbikitsa m’kabuku kakuti , Pamene Munthu Amene Mumakonda Amwalira . Koma koposa zonse , timafuna kukondedwa ndi Yehova . Conco , ngati inu ndi ine tanena fanizo limeneli mosavuta , n’cifukwa ciani Yesu , Mphunzitsi Wamkulu , sanagwilitsile nchito fanizo lofanana ndi limeneli ? Kucita izi kumaonetsa kuti timawakonda na kuwalemekeza . Ahabu anadzicepetsa , ndipo kucita zimenezi si cinali cinthu copepuka kwa munthu wonyada ndi wodzitukumula ameneyo . Cifukwa cakuti zinakana kuloŵelela m’ndale . Kundendeko sanali kulola ngakhale acibale ao kudzawaona . ( Mlal . 8 : 11 ) Kuonjezela apo , anthu amene amacita macimo koma safuna kulapa amakhala ngati “ miyala ikuluikulu yobisika m’madzi ” ndipo angaononge cikhulupililo ca ena mumpingo . — Yuda 4 , 12 . Zili ngati mmene timacitila na moto . Timausonkhela kuti upitilize kuyaka . Mlongo wina wokamba citundu ca Cixhosa , dzina lake Noma , poyamba anali kuyopa kuitanila abale aciyela a mpingo wa Cizungu kunyumba yake yosaukila . Tiyelekeze kuti Eodiya anaitana abale na alongo kunyumba kwake kuti akadye nawo cakudya na kusangalala ndi maceza . Mulungu anali kukondwela kwambili ndi iye . M’bale Mumba : Timakhulupilila kuti kugwilitsila nchito dzina la Mulungu , Yehova monga mmene Yesu Mwana wake anacitila ndi cinthu cofunika . M’bale wina anawauzanso kuti : “ Kuti mudziŵe ngati mupita patsogolo kuphunzila cinenelo musaziyelekezela zimene mwaphunzila tsiku lililonse , koma muzicita zimenezo pakapita miyezi ingapo . ” Danieli sanauzidwe tsiku limene adzaukitsidwa , kapena kutalika kwa nthawi imene idzapitapo kuti aukitsidwe . Ganizilani cimene cipangitsa mfundoyo kukhala yokopa , cifukwa cake ni yabodza , ndi zimene mungacite kuti mupewe kutengela maganizo aconco . Ndithudi , tonse tingakwanitse kupewa kutengela maganizo a dziko mwa kumvela mau amene Paulo analembela Akhristu a ku Kolose . Muziyamikila Mphatso Yanu ya Ufulu Wosankha Zocita , Jan . N’zoonekelatu kuti Elisa sanaganize kuti tsopano wadziŵa zonse . Esitere Tikamacita zimenezi ndiye kuti tikugwilitsila nchito mfundo zimene taphunzila m’fanizo la Yesu la mwana wolowelela . Kodi makolo acikhristu angaphunzitse bwanji ana awo ngati mnzawo wa m’cikwati si Mboni ? Mukatelo , iye adzaphunzila kudzipangila zosankha . N’cifukwa ciani atumiki a Yehova ayenela kukwatila ndi kukwatiwa kokha “ mwa Ambuye ” ? Paulendo wake waciŵili mu May 1903 , misonkhano yapoyela imene inali kucitikila ku Belfast ndi ku Dublin , inali kulengezedwa m’manyuzipepala . Koma ngati tiyesetsa kuthandiza ena , tidzapeza cimwemwe coculuka podziŵa kuti Mfumu ya cilengedwe conse ikukondwela nase . Ine ndikumudziŵa . ” Yankho lipezeka pa Chivumbulutso 20 : 7 - 15 . Kodi nanunso mumamva conco ? Nthawi zambili timamva mofanana ndi mtumwi Paulo amene anakamba kuti : “ Ndimafuna kucita zabwino , koma sinditha kuzicita . ” — Aroma 7 : 18 ; Yakobo 3 : 2 . Kumbukilani kuti patsiku la ubatizo wanu munafunsidwa mafunso pamaso pa mboni zambili . Munafunsidwa ngati munadzipeleka kwa Yehova ndi ‘ kuzindikila kuti kudzipeleka kumene munacita , ndi kubatizidwa kwanu , zinakupangitsani kukhala mmodzi wa Mboni za Yehova , wogwilizana ndi gulu la Mulungu limene amalitsogolela ndi mzimu wake . ’ 3 : 13 . Ndipo cikondi cimene ise na Akhristu anzathu tili naco pa Yehova cili ngati comangila cotigwilizanitsa pamodzi kwambili . M’kupita kwa nthawi , mabuku ena a m’Baibo anamasulidwa m’zinenelo zina zofala , monga Cisiriya , Cigotiki , ndi Cilatini . Mlongo wina dzina lake Grethel anati : “ Ndinavomela kukatumikila kudziko lina cifukwa ndi njila imodzi yoonetsa kuti ndimakonda Yehova , osati kukonda kwambili dziko , nyumba , kapena udindo winawake . ” Ni nchito yanji imene Yesu anapatsiwa imene pambuyo pake anasiila otsatila ake ? Izi n’zimene Yesu anacita pamene anali kuyambitsa mwambo wa Cikumbutso ca imfa yake , cimene cimachedwanso kuti “ Cakudya Camadzulo ca Ambuye . ” ( 1 Akor . ( Salimo 49 : 8 ) Pa cifukwa cimeneci tinali ofunikila thandizo locokela kwa Mulungu kuti timasuke mu ukapolo wa ucimo na imfa . 13 ‘ Kuika Maganizo Athu pa Zinthu za Mzimu Kumabweletsa Moyo na Mtendele ’ Poyamba Sauli anavalika Davide zovala zake zankhondo . 13 : 16 ) Aphunzitsi odzipeleka amenewo amakhala osangalala kwambili akaona kuti ophunzila akugwilitsila nchito luso lao potumikila mpingo . — Mac . 20 : 35 . Mwacitsanzo , anaphunzila kulalikila uthenga wabwino mogwila mtima ndi kukhala wokhulupilika panthawi ya mayeselo . Marilyn anafotokoza kuti : “ N’zosatheka kukumbatila mwana wako pa intaneti kapena kupita kukamugoneka . ” Kodi coonadi ca m’Baibo cili ngati lamba ya msilikali waciroma m’njila yotani ? Kenako , Chris anauza Gavin kuti maulosi a m’Baibulo ndi amene anamuthandiza kukhulupilila kuti Baibulo limakamba zoona . Muganiza kuti Bezaleli ndi Oholiabu anamva bwanji pa nthawiyo ? Van Amburgh , mkulu wa asilikali dzina lake James Franklin Bell wa ku America , anakamba kuti Dipatimenti Yoona za Cilungamo ku America inafuna kukhazikitsa lamulo lakuti munthu amene wakana kupita kunkhondo , aziphedwa . Kusintha kumeneku kungakhale kovuta . Yehova amafuna kuti atumiki ake onse azikhululukilana ndi kukhala mwamtendele . Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Kapolo wa Ambuye sayenela kukangana ndi anthu , koma ayenela kukhala wodekha kwa onse . ” Daniel anati : “ N’naona kuti nifunika kusintha zambili paumoyo wanga . ” Tonsefe ndife ocimwa ndipo tinatengela kupanda ungwilo kwa Adamu . 13 : 8 ; Mat . A Yohane : Tsopano ndaona kuti m’Baibulo muli zambili kuposa zimene ndinali kudziŵa . Iwo amakamba kuti mau amenewa aonetsa kuti Mulungu anaikilatu nthawi imene munthu aliyense adzafa . “ Mwa cikhulupililo , Mose atakula anakana kuchedwa mwana wa mwana wamkazi wa Farao . ” ( Chiv . 6 : 1 , 2 ; 13 : 1 - 18 ; 19 : 11 - 21 ) Kwangotsala kanthawi kocepa kuti zimenezi zicitike . Kodi mzimu wa Mulungu ungatithandize bwanji kupeza mtendele ? Mofananamo , ngati Mkristu mnzathu wafooka cifukwa ca mavuto aumwini , coyamba tiyenela kupeleka thandizo la kuuzimu . — Ŵelengani 1 Atesalonika 5 : 14 . Abisalomu anamvela malangizo a Husai osati a Ahitofeli . — 2 Samueli 15 : 31 ; 17 : 14 . Kodi kufuna udindo mumpingo n’kulakwa ? Kudzicepetsa kungatithandizenso kupanga zosankha zabwino ngakhale pamene sitidziŵa mmene zinthu zidzakhalila . Conco , kuti tipitilize kukhala maso mwauzimu , tiyenela kupemphela kwa Yehova nthawi zonse . — 1 Pet . 4 : 7 . Zaka 1,000 zapitazo , aphunzitsi odziŵa bwino Malemba analipo . Mwacitsanzo , lemba la Yesaya 54 : 17 limati : “ Cida ciliconse cimene cidzapangidwe kuti cikuvulaze sicidzapambana . ” Kumeneko anaona mapu a magawo ena akuluakulu a m’dzikolo amene kulibe alaliki . Ndi mwai waukulu kulambila Yehova mlungu uliwonse . Yehova watipatsa ufulu wosankha . Komabe , zinali zovuta kupita ku misonkhano ya pa Ciŵelu madzulo , popeza unali mtunda wa makilomita 10 , ndipo nthawiyo ndi imene tinali kufunika kukama mkaka ku ng’ombe . Kucokela pamene Ufumu unakhazikitsidwa mu 1914 , Yesu wakhala akukonza zinthu kuti atumiki a Mulungu akhale oyenelela kucita cifunilo ca Atate wake . 19 : 17 ; Aheb . 12 : 12 ) Mwacitsanzo , tingauze m’bale amene wakamba nkhani mmene nkhaniyo yatithandizila panthawi yake , kapena mmene watithandizila kumvetsetsa lemba lina lake . Nowa ayenela kuti anaphunzilanso kwa ambuye ake , a Metusela , ndi kwa a Yaredi , ambuye awo a ambuye ake . A Yaredi anakhalabe na moyo kwa zaka 366 kucokela pamene Nowa anabadwa . Ndinali kudziŵa kuti akhoza kutisamalila nthawi ina iliyonse . ” Kodi Aisiraeli ena anazindikila bwanji mphamvu za Mulungu ? Lembani makhalidwe a mnzanu wa m’cikwati amene mumakonda . Pangani Zosankha Mwanzelu Mukali Acinyamata Masiku ano , tiyenela kupeza mipata ya mmene tingathandizile Akristu okalamba kapena odwala . mau otanthauza tsunami m’cinenelo cao . Ena ni amanyazi ndipo amaopa kuti akaitana munthu ku nyumba kwawo adzasoŵa nkhani zoceza naye . Ndipo ngati zosankha zake zamubweletsela mapindu cifukwa cosankha mwanzelu , amaonetsa kuti wapeza nzelu zopindulitsa . Mboni zokhulupilika zinapitilizabe kumvela Yehova , ndipo iye sanazisiye . ( Mateyu 5 : 11 ; 11 : 19 ; Yohane 10 : 19 - 21 ) Motelo , ngati mukhala anzelu ndiponso osamala , mudzatha kuzindikila mabodza amene wina akukamba n’colinga cakuti asoceletse ena . — Miyambo 2 : 10 - 16 . Anthu m’maiko ambili amafuna kukhala omasuka ku mavuto monga umphawi , tsankho , na kupondelezedwa . Koma zimene anapeza m’mabwinja a Yeriko n’zosiyana ndi zimenezi . Kunena zoona , mphatso zimenezi zimaonetselatu kuti Mlengi wathu amatiganizila , ndi wacifundo ndiponso woolowa manja . Ngakhale kuti anatopa , sanabwelele m’mbuyo . Komabe , sanakwanitse kupeza nchito ya maola ocepa imene anali kufuna . Anthu ambili angakambe kuti Cingelezi ndi cofala kwambili . Akulu anathandiza banjali mwa kuwafotokozela citsanzo ca Yesu . ( Miy . 16 : 18 ) Ngati muli na udindo mu mpingo , umene ungacititse kuti ena azikulemekezani , muyenela kukhalabe wodzicepetsa . Iye amadziŵa mmene cibadwa canu , kukula kwanu , malo amene mumakhala ndi cikhalidwe canu zimakhudzila umunthu wanu . Amayesa njila izi na izi kuti apeze mtendele , pamene ise tili nawo kale . Nikolai Chimpoesh Ndiye cifukwa cake anakamba kuti : “ Zakwanilitsidwa ! ” Tsiku lililonse ndimayamikila Yehova cifukwa cokhala mu utumiki wanthawi zonse . ” ( Onani bokosi lakuti “ Zimene Zingakuthandizeni Kupita Patsogolo . ” ) Musagwe mphwayi ! Mwacitsanzo , Baibulo limakamba za kukhulupilika kwao , cikondi cao , zolakwa zao , ndi kusakhulupilika kwao . 1 : 23 ) Koma m’masomphenyawo , Yohane anaona anthu ena amene sali m’gulu la mkwatibwi . Iwo anatilanda njinga , katundu , makatoni a mabuku ndi mafaelo a dela . Koma ali wacinyamata , anakopeka ndi makhalidwe a m’dzikoli . Iye anam’sankha kukhala mtumwi , ndipo Natanayeli anakwanilitsa udindo wake mokhulupilika . ( Numeri 11 : 6 ) Pambuyo pake io anakamba mokwiya kuti : “ Cakudya conyansaci cafika potikola . ” Ngakhale ataloŵa m’banja komanso kukhala ndi ana aŵili , Mike sanasinthe colinga cake . Anafotokozela ana ake , wina wa zaka 8 wina 10 , za cifungadziko ( atmosphere , ndiwo mpweya wozungulila dziko lapansi ) , na kuwaonetsa mmene Yehova amatisamalila potiikila cifungadziko . Cifukwa ca ziphunzitso zimenezi , anthu ambili padziko lapansi amakhulupilila kuti imfa imatsegula nkhomo yoloŵela ku moyo wina . Ndi njila yabwino iti imene tingathandizile atumiki anthawi zonse ndi makolo ao ? Komabe , ena amaonetsako cidwi pang’ono . Tikagwela m’chimo lalikulu , tifunika kulapa moona mtima ndi kupempha cikhululukilo ca Yehova . Mphatso ya cimwemwe . POKHALA mnyamata woopa Mulungu , atate , a Arthur , anali n’colinga codzakhala m’busa wa chechi ca Methodist . Mphatso imeneyi ndi yapamwamba kwambili cakuti sitingathe kuifotokoza . Conco , ndi bwino kukamba nao mokoma mtima , koma mosapita m’mbali . Kupatsa ena mwa njila imeneyo kumanibweletsela cimwemwe . N’cifukwa ninji Mulungu anathandiza akazi a makolo akale okhulupilika amene anali kuopa Yehova ? M’nkhani ino , tidzakambilana zimene tingacite kuti tipewe kutengela maganizo a anthu a m’dzikoli . Iwo anauzidwa kuti M’bale Rutherford akakamba kaciŵili mau akuti “ Lengezani ! ” Kodi n’zoona kuti munthu akhoza kudziŵa zabwino na zoipa popanda kukhulupilila Mulungu ? Fotokozani . 5 : 23 ; Yoh . 2 : 3 - 11 ) Koma kodi Yesu na Paulo basi nthawi zonse anali kumangokamba za vinyo na kumautamanda ? ( Yoswa 9 : 3 , 9 , 10 ) Anacita bwino kuzindikila kuti Yehova anali kumenyela nkhondo Aisiraeli . Muzisintha - sintha kaŵelengedwe kanu . Alexandra anali khale pa mpando m’basi , ndipo anamvela munthu wina akukamba mau amenewa panja . Alexandra anali kuyembekeza kuti adutse malile a maiko aŵili a ku South America . Nili na zaka 29 , n’navulala kwambili pamene n’nali kufuna kugwila bola poseŵela . Panthawiyo , izi zinali zosatheka m’masukulu kapena m’mayunivisite ena . Iye adzakuthandizani monga mmene anathandizila Akristu akale amene anali kukamba nkhani za m’Sukulu ya Ulaliki . ​ — Ŵelengani Salimo 32 :⁠ 8 . Ngakhale n’conco , ife tonse timafunika kusankha pankhani yolinganako na imeneyi . Taona kuti kusilila kwa nsanje n’kulambila mafano . Koma kukali zaka 69 kuti Nowa abadwe , ‘ Mulungu anam’tenga ” Inoki . — Gen . N’ciani cimene cinali capadela kwa Debora ndi Yaeli ? Mukadziŵa nchito zimene zimapezeka kwanuko , muyenela kupeza malangizo amene angakuthandizeni . “ Uzikwanilitsa malonjezo ako kwa Yehova . ” — MAT . 6 : 24 . Baibo ni yosiyana kwambili na mabuku ena . MFUMU SOLOMO mouzilidwa analembela acinyamata kuti : “ Kumbukila Mlengi wako Wamkulu masiku a unyamata wako , asanafike masiku oipa . ” Izi n’zimene ine nakhala nikucita ndipo napindula ngako . Kuti adzipatsa anchito ake apakhomo “ cakudya pa nthawi yoyenela . ” Kodi “ anthu odziŵika ndi dzina lake ” amene Yakobo anakamba pa Machitidwe 15 : 14 , ndani ? Tingathe Kupewa Ciwelewele Komabe , kuŵelengela anthu Baibo tikakhala muulaliki , pakokha si kokwanila . Pakuti ine , Yehova Mulungu wako , ndagwila dzanja lako lamanja . Ine amene ndikukuuza kuti , ‘ Usacite mantha . Munthu anali kuika m’gulaye mwala wosalala wolemela mwina magalamu 250 . Mwacitsanzo , Mulungu anacititsa Nowa kukhala womanga cingalawa , anacititsa Bezaleli kukhala mmisili waluso , anacititsa Gidiyoni kukhala wolimba mtima pa nkhondo , ndipo anacititsa Paulo kukhala m’mishonale PADZIKO lapansi pali gulu la anthu amene amakonda Yehova ndi kum’tumikila . Pambuyo poukitsidwa , iye anakamba kuti : “ Ulamulilo wonse wapelekedwa kwa ine kumwamba ndi padziko lapansi . . . . Wamasalimo anaimbadi mokongola kuti : “ Yamikani Yehova anthu inu , pakuti iye ndi wabwino . Kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale . ” ( Sal . Ngati zimenezi zikukhudzani , yesetsani kukhalabe ndi maganizo oyenela . Mipukutu yofukulidwa m’matongwe ionetsa kuti Ayuda ambili anaphunzila zamalonda kumeneko , ndipo ena anakhala akatswili a zopanga - panga . Ngati Mkhristu waona kuti mnzake wamulakwila , ayenela kusamala kuti asayambe kumunenela misece . Posacedwapa , Mulungu adzaononga dziko loipali pa “ cisautso cacikulu . ” Mzinda wakumwamba umenewu uli ndi “ ulemelelo wa Mulungu , ” ndipo ndi “ wonyezimila ngati mwala wamtengo wapatali kwambili , ngati mwala wa yasipi wowala mbee ! ngati galasi . ” ( Chiv . Ngati musunga cakukhosi , mungaononge thanzi lanu komanso cikwati canu Kuganizila zolakwa zimene anthu ena anacita , kungatithandize kupewa kucita zolakwa zofananazo . Koma m’Baibo muli ulosi wina wocititsa cidwi wokhudza mfumu ya ku Perisiya , umene unakwanilitsidwa ndendende monga mmene unakambila . Masiku ano , padziko lapansi palibe kacisi weniweni amene ndi cimake ca kulambila koona . 17 N’cifukwa Ciani Kudzicepetsa N’kofunikabe ? Kuganizila mfundo ya palembali kungatithandize kupeza mayankho pa mafunso monga awa : ‘ Kodi nifunika kucita maphunzilo apamwamba ? Sitidziŵa zinthu zonse zimene Mariya anali kuda nazo nkhawa , koma tidziŵa zimene anayankha Gabirieli . Kodi kudzicepetsa kungatithandize bwanji kukhala okhutila ndi acimwemwe pamalo alionse amene tilipo ? Ofalitsa Ufumu ambili azindikila kuti ayenela kukhala ndi zolinga zoyenela kuti aonjezele cangu cao mu ulaliki . Koma kodi izi n’zoona ? ( Miyambo 27 : 11 ) Tangoganizani ! Timatha kum’kondweletsa Atate wathu wacikondi wakumwamba pamene tipanga zosankha mwanzelu , zozikidwa pa mfundo za m’Baibo . Mofanana ndi Yesu , timalalikila uthenga wabwino wa Ufumu . ( Mat . 6 : 14 , 15 ) Kodi muona kuti mufunika kuwongolela pa nkhani ya kuleza mtima , kapena kulamulila mkwiyo wanu ? Funso yacitatu idzayankhiwa mu nkhani yotsatila . ( Mlal . 5 : 4 ) Yesu nayenso anaonetsa kuti kupanga malonjezo ni nkhani yaikulu . ( Ŵelengani Maliko 12 : 29 , 30 ) Mwina pambuyo pokambilana mungapeleke pemphelo , ndi kupempha Yehova kuti apatse wophunzilayo mzimu woyela kuti umuthandize kugwilitsila nchito zimene adzaphunzila . Masiku ano , timalambila Yehova mwa kupemphela , kulalikila , ndi kupita kumisonkhano . Anali kugwilitsidwa nchito kuphimba macimo a anthu , amene anali kufuna kuti Yehova awakhululukile . Udzakhala wokondweletsa kwambili . 10 : 24 , 25 ) Aisiraeli anali kusonkhana kuti amvetsele ndi kuphunzila za Yehova kotelo kuti azimuopa ndi kutsatila Cilamulo cake . ( Deut . Tikuphunzilapo kuti wacinyamata wofikapo mwakuuzimu angakhale wokhulupilika ngakhale pa nthawi yovuta . Akulu amenewa si “ olamulila ” cikhulupililo ca ena , koma ni ‘ antchito anzathu ’ amene amatithandiza kukhala na cimwemwe . — 2 Akor . N’nakhala na mwayi wothandiza banja lina kuphunzila coonadi m’gawo limene kunalibe mpingo . ” “ N’taona kukula kwa Baibo , cilakolako cofuna kuiŵelenga cinasila . ” — Ezekiel Simon anacita khama kuphunzila cinenelo ca Cipalau , ndipo zimenezo zinam’thandiza ‘ kufutukula mtima wake ’ kwa abale ndi alongo a kumeneko . ( 2 Akor . Ndiyeno , n’nazindikila kuti panjapo panali pozizila kwambili ! Musalole kuti zokamba kapena zocita za ena zikufooketseni ndi kucititsa kuti musakhale maso . Paul Mu umoyo wanga wonse , sin’naonepo anthu abwino conco ngati awa . ” Tiyeni tikambilane mafunso amenewa . Kuŵelenga ndi kuphunzila kungakuthandizeni kukhala wosangalala ndiponso kutulukila zinthu zina . Tikadzipeleka kwa Yehova , timamuuza kuti , “ Ndakupatsani moyo wanga . ” Pamatenga nthawi kuti munthu akhulupilile zimene amaphunzila . Kodi mbili ya anthu yaonetsa ciani ? Kaya Ni pa zocitika zina ziti pamene Yehova waonetsa kudziletsa ? Kodi Mulungu adzakwanilitsa bwanji colinga cake kwa anthu ? Zinthu zambili zimene tinaona na kucita ku United States zinali zacilendo kwa ise . Pa cifukwa ici , n’nali kupempha madalaiva a mathilaki kuti anilole kukwelako pamwamba pa vimitengo vimene anali kunyamula pa mathilakiwo . Atayenda kamtunda ndithu , mzinda wa Lusitara umene uli pamwamba pa phili , uyamba kubisika . M’Mabaibulo ena a Cingelezi munalinso zophophonya zofananazo . Poona mmene bongo wathu ndi thupi lathu zinapangidwila , ambili azindikila kuti pali Mlengi wanzelu amene anatipanga . M’malo mwake , Adamu anali kudziŵa kuti akamvela lamulo la Mulungu lakuti asadye cipatso coletsedwa adzakhala kosatha , kutanthauza kuti iye sadzafa . Uziopa Yehova ndi kupatuka pa coipa . ” Panthawi iyi , Yehova anam’lonjeza cinthu cosangalatsa kuti : “ Ndidzatulutsa mtundu waukulu mwa iwe . ” Mwa kucita zimenezi caka ciliconse timasonyeza kuyamikila cikondi cimene Mulungu ndi Yesu anationetsa . — Ŵelengani Luka 22 : 19 , 20 . Onani kuti lembali lionetsa kuti mtendele umenewu udzakhalapo “ cifukwa dziko lapansi lidzadzaza ndi anthu odziŵa Yehova . ” ( Yes . Mau a m’Baibulo akuti “ akuyesetsa ” anamasulilidwa kucokela ku mau a Cigiliki amene amatanthauza kufunitsitsa , kapena kukalamila . “ Yehova Amadziŵa Anthu Ake , ” 7 / 15 Anthu ena angakhudzike mtima akamvela mmene Baibulo imakambila zoona pa maulosi ndi mbili yakale . “ Ndidzakupatsa malangizo ndi kukuyang’anila . ” — SAL . Mkazi wanga anayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . 18 , 19 . ( a ) N’cifukwa ninji nthawi zina Akristu okalamba sangadziŵe mmene citsanzo cao cimalimbikitsila ena ? Conco tisanayambe kuŵelenga Baibulo , tiyenela kupempha Yehova kuti atithandize kukhala ndi maganizo oyenela , tingam’pemphe kuti atipatse nzelu kuti timvetsetse zinthu zimene afuna kuti tidziŵe . — Ezara 7 : 10 ; ŵelengani Yakobo 1 : 5 . Koma uthenga wa m’Baibulo sunasinthe . Mukangolandila maudindo mumpingo musaganize kuti tsopano mufunika kusintha zinthu zonse . Musasinthe zinthu cifukwa cofuna kungotsatila zofuna zanu koma cifukwa cofuna kusamalila bwino mpingo ndi kutsatila malangizo amene gulu la Yehova limapeleka . Zimanipangitsa kukhala bize podziŵa kuti nifunika kukwanilitsa colinga cina cake . Pamene Yesu anali pa dziko lapansi , amuna aciyuda anali kusudzula akazi awo mwaciwembu “ pa cifukwa ciliconse . ” ( Mat . Tinali kutangwanika kwambili ndi nchito yosamalila ziŵeto . Davide analinso wacifundo . Pofotokoza fanizo lake lothela la nkhosa ndi mbuzi , Yesu analunjika mfundo yake kwa anthu amene ali ndi ciyembekezo ca padziko lapansi . Mashelufu a mawilo , matebulo , ndi zinthu zina zoikapo mabuku zinagulidwa kudzela mu ofesi ya nthambi ya ku Hong Kong ndi kutumizidwa padziko lonse Kodi kudzicepetsa kudzatiteteza bwanji pa zocitika zaconco ? ( Mlal . 3 : 7 ) Koma zimenezi sizitanthauza kuti tiyenela kusiya kulankhalana ndi mnzathu wa mucikwati cifukwa kulankhulana kumathandiza cikwati kukhala colimba . Pamene bwenzi lathu lasintha khalidwe lake mwadzidzidzi , tikhoza kudabwa . Kaya mucita homuweki , mugwila nchito za pakhomo , kapena mugwila nchito ina iliyonse yakuthupi , muziicita ndi mtima wonse . ( Yuda 11 ) Mwacitsanzo , iye angalole maganizo a ciwelewele ndi a dyela kuzika mizu mu mtima mwake . Kapena angayambe kusungila Mkhristu mnzake cidani . ( 1 Yoh . Ngakhale n’conco , kuganizila zimene zingacitike kungathandize acibale a wodwala kucepetsa mantha na kuika maganizo awo pa zinthu zimene zingawakhazike mtima pansi . Kodi pali ciyembekezo canji cokhudza okondedwa anga amene anamwalila ? Komanso , anthu sangafotokoze cifukwa cake timalaka - laka kukhalabe na moyo osafa . ( Mlal . 10 : 22 - 26 ; 3 Yoh . 9 , 10 ) Koma tifunika kuyesetsa kutsatila mfundo za m’Baibo pa nkhani ya kulemekeza ena . ( 2 Tim . 3 : 1 ) Nkhani yaciŵili idzafotokoza mmene makhalidwe a anthu m’masiku otsiliza ano alili osiyana kwambili na makhalidwe a anthu a Mulungu . Frieda , amenenso ali na zaka za m’ma 20 anakamba kuti : “ N’nali kukwiya msanga . ( Ezara 4 : 1 - 4 ) Mu 522 B.C.E . , nchito yomanga ku Yerusalemu inaimilatu cifukwa mfumu ya Perisiya inapeleka lamulo loletsa nchitoyo . Mwana akalimbikitsidwa , amadziona kukhala wofunika . ” 7 : 13 , 14 ) N’zosacita kufunsa kuti Yehova amadalitsa khama la conco . Mu October 1927 , Ophunzila Baibulo anakonza zakuti nkhani za m’Baibulo zizipelekedwa m’tauni ya Tokyo . FARAO anali mfumu yamphamvu ndipo Aiguputo anali kumuona ngati mulungu wamoyo . Julio , * amene anatumikila monga mkulu ku Bolivia kwa zaka zoposa 20 , anati : “ Kukonzekela nkhani , kucezela abale , ndi kucita maulendo aubusa inali mbali yaikulu ya moyo wanga . ( Yak . 3 : 17 ) Ngati tikhala amtendele ndi ololela , timaonetsa kuti tili na nzelu zaumulungu . Iye analemba kuti : “ M’masiku amenewo , amuna 10 ocokela m’zilankhulo zonse za anthu a mitundu ina adzagwila covala ca munthu amene ndi Myuda ndi kunena kuti : ‘ Anthu inu tipita nanu limodzi , cifukwa tamva kuti Mulungu ali ndi inu . ’ ” ( Zek . ( Yobu 31 : 1 ) Tikamacita zinthu mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu , tidzaphunzila ‘ kunyansidwa ndi coipa ’ ndi ‘ kugwilitsitsa cabwino . ” — Aroma 12 : 2 , 9 . 15 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi ( b ) N’cifukwa ciani mkwiyo wa Mulungu sunamugwele Hezekiya ? Kodi Anthu Adzaononga Dziko Lapansi Kothelatu ? — November - December Danieli 4 : 13 - 17 . Apainiyawo anadalitsidwa cifukwa ca khama lawo pamene anakumana ndi maneja wa hotela ina m’tauni yochedwa William Creek , ku sitesheni ya sitima . Ndalama zake zinamuthela . UCIFWAMBA : Lipoti ionetsa kuti zigaŵenga zoposa 30,000 zimavutitsa anthu ku United States . Ndi maumboni otani amene tili nao oonetsa kuti Yehova amatikonda ? Mtumwi Paulo atakamba kuti masiku otsiliza ano adzakhala “ nthawi yapadela komanso yovuta , ” anauzilidwanso kulemba kuti : “ Anthu oipa ndi onyenga adzaipilaipilabe . ” ( 2 Tim . Martin Luther mtsogoleli wa gulu lotsutsa Cikatolika ku German anacha apapa Acikatolika kuti okana Kristu . ( a ) Ndi madalitso ati amene adzacititsa umoyo kukhala wosangalatsa m’dziko latsopano ? Ngati palinso cinthu cina cimene cakhala cofunika koposa kwa ine , ndico kumamatila ku gulu la Yehova looneka . ( Gen . 6 : 4 , 5 , 11 ; Yuda 6 ) Koma Yehova anamuuza mau amene anamulimbikitsa kupitiliza ‘ kuyenda ndi Mulungu . ’ ( b ) Kodi m’bale wina anaphunzila bwanji kulimbikitsa mgwilizano mumpingo ? Ngati mwadziŵa munthu wokhudzidwa ndi nkhaniyo , kodi mudzacita mwanzelu ndi kupewa kuyanjana ndi munthu ameneyo ? Anamuuza uthenga wakuti alengeze kwa anthu a m’nthawi yake . N’cifukwa ciani n’zomveka kukamba kuti alambili a Yehova ni olinganizika mwadongosolo ? Koma anayamba kutsatila zimene anaphunzila m’Baibo . Tikatelo , timaonetsa kuti tikufunitsitsa kukhala anthu auzimu ? — Mlal . Cifukwa cokhulupilila zimenezi , timasiyana na Asaduki , amene anali kukanilatu za kuuka kwa akufa . Conco palipano , palibe munthu amene angapewe mavuto amenewa . Koma anakondwela ndi Yobu , ndipo anamucha “ mtumiki ” wake . N’cimodzi - modzinso masiku ano . Ngakhale n’conco , mikangano pakati pa Akhristu ikhoza kubuka cifukwa ca kunyada ndipo ingafike poipa kwambili . 4 Ziphunzitso za m’Baibo N’zothandiza Nthawi Zonse Mosiyana ndi dzikoli , Yehova amafuna kuti tikhale ndi cidziŵitso , ndipo amatithandiza kukhala anzelu . Zolakwa zanga zandikulila . Inu mudzatikhululukila macimo athu . ” — Sal . Ndiye anapempha mnzake kuti : “ Usayambe zonifunsa kuti nanga iwe uganiza ciani , ungoniuza cabe zocita . M’mipingo yoposa 110,000 padziko lonse mukucitikanso nchito imene anthu ena sadziŵa zolowetsedwamo . Komabe , Sara analimba mtima , ndipo tsiku na tsiku anali kukonzekela ulendo wawo . Kodi Ufumu wa Mesiya n’ciani ? Nanga ndani amene Yehova wamuika kukhala Wolamulila mu Ufumuwo ? CIFUKWA CAKE ENA AMAKAIKILA : Ngakhale pamene afunikila kwambili cilimbikitso , anthu ena amaona kuti ndi kudzikonda kupempha Mulungu kuti awathandize kupilila mavuto ao . TSAMBA 24 • NYIMBO : 103 , 66 Mboni zambili zinatengedwela kupolisi kuti zikafunsidwe mafunso . Ndiyeno , ikani maganizo anu pa zimene mwana wanu akamba , pofuna kuonetsa kuti mukuziona kukhala zofunika , olo kuti zioneke monga n’zosafunika . ( Yakobo 5 : 11 ) Tiyeni tikambilane zitsanzo zoŵelengeka za anthu amene anapilila . — Onani mau akumapeto . Mosiyana ndi zimene ambili amaganiza , kodi n’ciani cofunika kuti anthu akhale na ufulu ? Tikamaphunzitsa bwino cikumbumtima cathu ndi kucitsatila , timakonda kwambili Yehova ndipo cikhulupililo cathu cimalimba ( Aroma 12 : 21 ) Zocitika zambili m’dziko lino la Satana n’zopanda cilungamo . Ophunzila Baibulo anali cabe 36 pamene anacita msonkhano wao waukulu woyamba m’tauni ya Kobe . ( Zek . Kuyambila m’nthawi ya atumwi , anthu a Mulungu akhala akucokela m’mitundu ndi m’zikhalidwe zosiyanasiyana , ndipo amachedwa Isiraeli wauzimu . Zotulukapo zake n’zakuti acicepele ndi acikulile omwe amayamba kutengela kavalidwe kawo , kakambidwe kawo , kapena zocita zawo . 8 , 9 . ( a ) Kodi tingakambitsilane bwanji ndi munthu amene amakhulupilila kuti Yesu ndi wolingana ndi Mulungu ? ( Gen . 2 : 18 , 24 ) Zaka 1,600 pambuyo pake , Yesu Khristu anaphunzitsa ophunzila ake kuti ayenela kutsatila mfundo zolungama zimenezi , zokhudza cikwati na kugonana . — Mat . Ngakhale kuti ‘ mitundu yonse imadana nafe , ’ malamulo a m’maiko ambili amatilola kulambila Yehova mwaufulu . — Mat . Iye angatitsogolele pogwilitsila nchito mzimu woyela . Ku Heburoni analamulila zaka 7 , ndipo ku Yerusalemu analamulila zaka 33 . ” Sinifuna zovutika n’kuganiza - ganiza . ” Titafika pa Nyumba ya Ufumu , ndinakana kukakhala kutsogolo m’malo mwake ndinakhala pafupi ndi khomo n’colinga cakuti ndiziona anthu otuluka ndi oloŵa . Conco , liu lakuti “ tiagalu ” liyenela kuti linapeleka cithunzi m’maganizo mwa mayiyo ca nyama yokondekayo . Pamene mucita zimenezo dzifunseni kuti , ‘ Sembe anthu amatsatila mfundo zimenezi , kodi dziko siikanakhala malo abwino ? ’ Conco , tanthauzo la maulosiwa linayenela kudziŵika mtsogolo , ‘ m’nthawi yamapeto . ’ Ganizilani zocitika zimene zingawalepheletse kucita zinthu zabwino , ndipo athandizeni kuzipewa . Muzicita zinthu zokuthandizani kuti mukule mwauzimu , komanso muziyesetsa kudziŵa na kutsatila malangizo atsopano a gulu . Mary anali ndi nchito yotaipa nkhani zophunzila mu Nsanja ya Mlonda ndi zofalitsa zina poseŵenzetsa ziwiya zina zolembela zimene zinathandiza kuti azilemba makope ambili - mbili panthawi imodzi . Yesu Kristu , Mfumu yathu akadzaonekela , tifunika tidzakhale pakati pa anthu amene adzalandila mphoto . Koma zimenezi zimawavuta . Ku Babulo wakale , anyamata atatu aciheberi anaponyedwa m’ng’anjo yamoto kuti afe , koma Mulungu “ anatumiza mngelo wake ndi kupulumutsa atumiki ake . ” — Danieli 3 : 19 - 28 . ( b ) Kodi pali lemba limene mumagwilitsila nchito limene lakhala ndi zotsatilapo zabwino ? Yehova waonetsa cikondi cake cacikulu m’njila zambili . Ngakhale n’telo , aliyense ali ndi udindo wosunga ubwenzi wapadela umenewu . Kodi mungakonde kuphunzila Baibulo panokha ? Wasayansi wina , dzina lake David Bodanis , anati : “ Mphamvu imene dzuŵa limatulutsa pa sekondi imodzi cabe ni yolingana na mphamvu ya mabomba [ a nyukiliya mabiliyoni ambili ] . ” Mosasamala kanthu za vuto limene Sylviana ali nalo , zimene anali kulaka - laka zinatheka . Ndipo anadalitsidwa kwambili . Nthawi zonse nimayamikila kuti iye sanaike maganizo ake pa colakwa cimene ine n’namucitila , koma anali kufuna kunithandiza kuti nisakumane na mavuto . Koma tili ndi zifukwa zomveka zokhulupilila kuti Yesu ali moyo , ndi kuti tsopano akutitsogolela pamene tilengeza uthenga wabwino padziko lonse . Linayamba kulembedwa mu 1513 B.C.E . , ndipo linatha mu 98 C.E . Linalembedwa kwa zaka zoposa 1,600 . Masiku ano , ndi mautumiki ati anthawi zonse amene mumayamikila ? ( Yak . 1 : 9 ) Ena akatikhumudwitsa , timayesa kuganizila zimene zawacititsa kukamba mau oipa kapena kuticitila zoipa . N’ciani cingatithandize kuti tiziona utumiki wathu moyenelela ? Titasonkhana , tinaimba nyimbo ya Ufumu , ndipo kenako tinamvetsela nkhani ya ubatizo . Koma timayembekezela kuti mtsogolo Mulungu adzathetsa matenda onse . ( Mat . 13 : 23 ) M’nkhani ino , tidzaona mmene kucita zimenezi kungakuthandizile kulimbitsa cikhululupililo cako mwa Mulungu Mlengi , na m’Mau ake Baibulo . Ndipo pali maumboni ambili otsimikizilika okhudza nkhani zimenezi . — Aheb . Conco , analeka kugwilizana ndi anzake oipa , kenako anabatizidwa , ndipo pambuyo pake anatumikila pa Beteli . KUDZILETSA N’ciani cingathandize acicepele ndi okalamba kukhalabe olimba panthawi zovuta ? Komabe , sikuti tifunika kuyembekezela dziko latsopano kuti tikasangalale ndi madalitso akuuzimu amene amabwela cifukwa cotumikila Yehova ndi mtima wonse . Ena aona kuti sangacitile mwina koma kupatukana pa zifukwa izi : kusasamalila banja mwadala , nkhanza zoipitsitsa , ndi ciwopsezo pa umoyo wauzimu . Koma sitingatsimikizile mfundo imeneyi , mwina akamba zoona . Tikacita zimenezo sitizayamba kudela nkhawa kwambili zinthu zimene timafunikila . Ananiika m’cipinda canekha kwa miyezi 6 . Umenewu ndi mwai wamtengo wapatali kwambili . — Mlaliki 3 : 11 . Kukamba zoona , kutumikila Yehova , Mulungu wathu wamkulu , kwanithandiza kukhala na umoyo wacimwemwe ndi waphindu . [ Caption on page 15 ] Kuyambila kumanzele : Poyamba nchito yolalikila siinali kupita patsogolo m’dzikolo . Yehova angakhale ndi zifukwa zomveka zimene sacitilapo kanthu . ( Gen . 6 : 8 , 9 , 14 - 16 ) Cingalawaci cinapangidwa m’njila yakuti ciziyandama pamadzi kuti anthu ndi nyama apulumuke . Nowa ndi banja lake anacita zonse zimene Yehova anawauza . Iwo anakumana na ziyeso zoopsa ngati “ moto . ” ( Mateyu 6 : 10 ) Ufumuwo ni boma imene idzalamulila dziko lonse lapansi , ndipo Mfumu yake ni Yesu Khristu . Polalikila m’gawo la anthu acikuda , nthawi zina tinali kugogoda pa nyumba ya azungu mosadziŵa . Akerubi nawonso ali paudindo wapamwamba , ndipo amasamalila nchito zapadela zokhudzana ndi ulemelelo wa Wamphamvuzonse . ( a ) N’ciani cimene Mfumu Hezekiya anacita ataukilidwa na Mfumu Senakeribu ya Asuri ? ( Maliko 4 : 35 - 41 ) Conco , mavuto onse amene amacitika cifukwa ca “ nthawi yatsoka ndi zinthu zosayembekezeleka ” adzatha . Pa mavuto amene anthu a m’banja amakumana nawo , pali vuto lina limene saliyembekezela . 11 : 19 - 21 ; 19 : 1 , 19 , 20 ) Cifukwa ca dalitso la Mulungu , Akristu amenewo anapita patsogolo kuuzimu . — Miy . Kenako Eliya anatengedwa mumphepo yamkuntho . Mkate Wamoyo , 6 / 1 Kulephela kutsatila malangizo ouzilidwa amenewa kungaononge ubwenzi wathu ndi Atate wathu wakumwamba amene ndi wolungama . Patapita zaka pafupifupi 100 mpingo wacikristu utakhazikitsidwa , mpatuko unabuka pakati pa Akristu monga mmene Malemba ananenela . ( Mac . Aliyense payekha afunika kuiganizila nkhaniyi . Ndiyeno m’Paladaiso pa dziko lapansi , anthu amenewo adzaphunzitsidwa cifunilo ca Mulungu . Citsanzo ca Davide , Mfumu ya Isiraeli wakale , cili ndi phunzilo lofunika . Ndipo anatithandiza , mogwilizana ndi zimene Yesu analonjeza . Mwana wa Sauli Yonatani , ndiponso mtsogoleli wa gulu lankhondo , Abineri , analipo pamene Davide anabweletsa mutu wa Goliyati kwa Mfumu Sauli . Kuti mudziŵe zambili , onani nkhani yakuti “ Kuthandiza Anthu Odwala MCS , ” mu Galamukani ! “ Cilengedwele dziko kupita mtsogolo , makhalidwe a Mulungu osaoneka ndi maso akuonekela bwino . . . m’zinthu zimene anapanga . ” — Aroma 1 : 20 . Poyamba , banjali linali kudziŵika kuti Abulamu ndi Sarai mpaka pamene Mulungu anasintha maina awo . Koma m’nkhani ino tidzaseŵenzetsa maina amene amadziŵika nawo kwambili . Mwacionekele , iye anadziŵa kuti angakumane ndi mavuto aakulu akakana kugona naye . Ine na mkazi wanga tikusangalala m’cikwati cathu cifukwa timayesetsa kutsatila kwambili malangizo a m’Baibo okhudza mabanja . Yesu anali kusangalala kuona anthu ofatsa akulandila uthenga wabwino . 20 : 26 , 27 ; Aroma 1 : 14 , 15 . Iye anafunika kuyang’ana kwa Yehova . — 1 Mafumu 19 : 14 - 18 . Coyamba , ganizilani za anthu amene akuchulidwa m’fanizoli . Mitu yabanja yambili yaona kuti kugwilitsila nchito magazini yokhala ndi cingelezi cosavuta imeneyi kwathandiza ana ao kuti azimvetsetsa kwambili Nsanja ya Mlonda . Buku lake la Yehova silipita m’mbali pankhani imeneyi . Aliyense amakhala na cidalilo cakuti olo pakhale mavuto , mnzawo wa m’cikwati sadzawasiya . Imeneyi ni cenjezo yamphamvu kwa ife ! ( Onani pikica pamwambapa . ) ( b ) N’ciani cingathandize acicepele acikhristu kupanga zosankha mwanzelu ? Pamene ndinali ndi zaka zisanu , ndinayamba kuphunzila kuvina . Ataphunzitsa mayi wina zinthu zokhudza kulambila koona , Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Cakudya canga ndico kucita cifunilo ca amene anandituma ndi kutsiliza nchito yake . ” ( Yoh . Tito anakhala mfumu mu 79 C.E . , kuloŵa m’malo atate wake , Vespasian . “ Mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu . ” — AFIL . Basi itaima , anthu anayamba kutsika . Sindiona kuti ndinalakwitsa kupanga cosankha cimeneci . ” Kodi nkhani ya m’Baibulo yokhudza Naboti inali kufotokozedwa bwanji m’nthawi zakale ? M’masophenyawo , Ezekieli si amene anali kuika cizindikilo kapena kupha anthu a mumzindawo . Mwacitsanzo , mtumwi Paulo pa maulendo ake a umishonale anapita ku dela limene lomba timati dziko la Turkey . * Kumeneko , iye anayesetsa kulalikila anthu ambili . ( Ŵelengani Mateyu 28 : 19 , 20 . ) Tsiku lina mumzinda wa Lusitara umenewo munabuka cipolowe . Nchito yomanga cihema itatha , “ mtambo unayamba kuphimba cihema cokumanako , ndipo ulemelelo wa Yehova unadzaza m’cihemaco . ” ( Eks . Inunso acinyamata , landilani maudindo , khalani odzicepetsa ndipo pitilizani kulemekeza acikulile . N’cifukwa cake n’kwanzelu kuti coyamba mupange zosankha pankhani zofunika kwambili . — Afil . Satana na ziwanda zake ali na makhalidwe oipa ndipo ndi ankhanza . Ambili amene tinali nao ku Gileadi analinso osakwatila . Ndisanacoke kumpingo wa Delray Beach ku Florida , ndinanyamula mabuku ambili m’galimoto yanga . Kenako ndinanyamuka ndi kulowela kumpoto mu mseu wochedwa Interstate 75 . Ndipo amaoneka kuti ndi wofunitsitsa kutumikila Yehova . ” Kodi Yehova anacita ciani ataona kuti anthu ake aleka kugwila nchito yake ? Simufunikila kucita kuyang’ana kutali kuti muone mavuto ndi zoipa zimene zaculuka masiku ano . Koma kuganiza conco n’kudzinamiza cifukwa tikhoza kutaya cinthu ca mtengo wapatali cimene ndi ubwenzi wathu ndi Yehova . N’ciani cinawathandiza kugonjetsa zopinga monga nyengo yovuta , komanso kuphunzila citundu na cikhalidwe catsopano ? Anali kupemphela kwa Yehova na kudalila thandizo lake . Nthawi zonse macimo a mtundu umenewu afunika kusamalidwa ndi akulu . Rabeka anali kuzidziŵa ngamila , koma sitidziŵa ngati iye anali kudziŵa kukwela pa ngamila . Takhala tikuŵelenga mobwelezabweleza malangizo opezeka pa lemba la Aheberi 10 : 24 , 25 . Dziko lapansi lidzadzala ndi ana ake amene adzakondwela kusamalila dziko lapansi ndi nyama . Abale acikulile safunika kukwinyilila kukakhala kofunikila kuti asiyile maudindo abale acinyamata . ( 1 Timoteyo 3 : 4 , 5 ) Kodi citsanzo ca mlongo Debbie ndi amuna ake cinathandiza bwanji banja lao ? Wonyamula zida zake ayenela kuti anathaŵa cifukwa ca mantha . ( Aheb . 7 : 11 ; 10 : 1 ) Ndipo kupyolela m’pangano limenelo , Aisiraeli anali ndi mwai wapadela wodzakhala “ ufumu wa ansembe , ” malinga ngati io akanamvela malamulo a Yehova . Monga taonela , Timoteyo , coyamba anali kudziŵa Malemba , ndipo caciŵili anakhulupilila zimene anaphunzila . Iwo amaganiza kuti anthu abwino amenewo safunika kucoka m’zipembedzo zonyenga ndi kuyamba kum’lambila monga anthu apadela . Iye sadzandisiya monga mmene mwamuna wanga anacitila . ” Iye anati : “ Pitilizani kuyenda mwanzelu pocita zinthu ndi anthu akunja . . . kuti mudziŵe mmene mungayankhile wina aliyense . ” — Akol . Yesu anakamba kuti : “ Mwakutelo , onse adzadziŵa kuti ndinu ophunzila anga , ngati mukukondana . ” Yesu anacha anthu omwe ali ngati nkhosa kuti ‘ olungama ’ cifukwa io amazindikila kuti Kristu ali ndi gulu la odzozedwa amene akali padziko lapansi , ndipo amathandiza odzozedwawo mokhulupilika m’masiku ano otsiliza . — Mat . Kodi mufuna kudziŵa za tsogolo lanu ? ( Luka 23 : 43 ) Kodi timamva bwanji kukhala ndi ciyembekezo cimeneci ? ( Chivumbulutso 6 : 5 , 6 ) Pa nkhondo yoyamba ya padziko lonse , anthu pafupi - fupi 750,000 anafa ndi njala ku Germany cifukwa ca mpanda umene adani anamanga pofuna kuti anthu a m’dzikolo asamatuluke . Mwacitsanzo , caka cina m’malanga , tinasoŵa ndalama zoyendela kupita ku msonkhano wacigawo . M’bale wina anavomela kugula motoka yathu kuti tipeze ndalama zoyendela . M’malo mokonda Mlengi wawo , ‘ amadzikonda ’ okha . ( 2 Tim . Pitilizani kupemphela kuti Mulungu akuthandizeni kujaila mu mpingo wanu watsopano . KUKOKA FODYA KUMAONONGA THUPI Buku lina lochewa The Tobacco Atlas linati : “ Asayansi anapeza kuti ngati munthu amakoka fodya , pafupifupi ziwalo zake zonse zimaonongeka ndipo nthawi iliyonse angadwale ndi kufa . ” Osati otsiliza dziko kapena anthu , koma mavuto amene avutitsa anthu kwa zaka masauzande na kupondelezewa . Iwo akadzayamba kulamulila dziko lapansi m’zaka 1,000 , anthu onse adzakhala otetezeka . Pa lembali pali makambitsilano amene Yesu anali nao ndi atumwi ake . Panthawi ina , iye anauza ophunzila ake kuti : “ Kwezani maso anu muone m’mindamo , mwayela kale ndipo m’mofunika kukolola . ” ( Yoh . Cosankha cimodzi cofunika kwambili cimene acicepele amafunika kupanga ndi cokhudza zolinga zawo . M’malo mocilikiza mokhulupilika Yesu ndi Ufumu wake , io amacilikiza maulamulilo a anthu ndiponso amaphwanya mfundo za m’Baibulo kuti akhale ndi mphamvu pandale . 3 Mbili Yanga ​ — Kucita Zimene Yehova Watilamula Kumabweletsa Madalitso Iwo anandiyamikila kwambili . ” Tikamasamalila Nyumba yathu ya Ufumu , timakhala omasuka kuitanila anthu acidwi kumisonkhano yathu podziŵa kuti Nyumbayo ndi yooneka bwino mogwilizana ndi uthenga umene timalalikila . Ngati mwaona kuti zimenezo sizicitika mwamsanga , pewani kuda nkhawa ndipo musataye mtima . Masiku ano , makolo ena analekelatu kupeleka cilango kwa ana awo kuopela kuti mwina angayambe kudziona osafunika . Anayamba kutifotokozela zimene amakhulupilila pogwilitsila nchito Baibulo . 28 : 16 ) Tiyeni tikambilane cifukwa cake fanizolo n’lofunika . Baibulo imakamba kuti nkhondo imeneyi inacitikila m’Cigwa ca Ela . 19 : 7 , 8 ; 21 : 9 ; 2 Akor . KULEMBEDWA KWAKE : Linalembedwa ndi amuna 40 kwa zaka zoposa 1,600 , kucokela mu 1513 B.C.E . mpaka ca ku ma 98 C.E . Komabe , popeza ndise opanda ungwilo , anthu akakwatilana n’kukhala na banja lawo , pamakhala mavuto ena amene angasokoneze mgwilizano wawo ndi acibululu awo . Caputa 4 ca buku limeneli la m’Baibo cimafotokoza cifukwa cimodzi cimene cipangitsa Yehova kukhala woyenela kulandila ulemu . Atafika kunyumba anapeza atate ŵake , a Jese , akamba na munthu wina wokalamba . Mphatso imeneyi ndi yamtengo wapatali kwambili cakuti sitingathe kuifotokoza mokwanila . 3 - 5 . ( a ) Kodi Asa anakumana ndi vuto lanji ngakhale kuti anali ndi mtima wathunthu kwa Yehova ? Mulungu ndi wolungama m’njila zake zonse.Iye ndi wolungama , wokhulupilika , ndi woongoka . Nanga n’ciani cinam’thandiza kuyembekezela moleza mtima ? Tsiku limenelo n’nakangiwa kugona usiku wonse . Amawakonzela zakudya , malo ogona ndi zina zofunikila . Franz ndi Margit anasamukila ku dela lina cifukwa ca utumiki ndipo sanapitilize kuphunzila ndi banja lija . Conco , si odzozedwa onse masiku ano amene ali mbali ya “ m’badwo uwu ” umene Yesu anachula . Conco , iye anapeleka cenjezo lakuti tiyenela ‘ kupewa ’ anthu amene ali na cikondi cadyela . ( 2 Tim . Nyimboyo inaimbidwa bwino kwambili . 40 : 5 ; Zek . Kumvela mwanjila imeneyi sikutanthauza kuti tilibe cikhulupililo , koma ni umboni wakuti nchito yolalikila timaikonda . M’bale wina m’dziko la Ghana , anagaŵila mnyamata wina cofalitsa . Ndiyeno mnyamatayo anayamba kubisala m’baleyo . Ngakhale zinali conco , iwo anali kutumikila pamodzi mwamtendele . ( Mac . Patapita mawiki aŵili , Riana ananyamuka ku delalo kupita ku msonkhano wa cigawo . Katswili wina wa mbili yakale , dzina lake Simon Schama , anakamba kuti dandaulo limeneli “ likutiphunzitsa zambili osati cabe zakuti munthu woseŵenza m’munda anali kucondelela kuti amubwezele [ covala cake ] . Kupatsa Kumapindulitsa , Na . Ganizilani citsanzo ca mtumwi Paulo . ( Luka 15 : 20 ) Komanso , makolo amenewo amakhalabe okhulupilika kwa Yehova , ndi kupemphelela kuti citsanzo cawo cabwino ciwatunthe anawo kubwelela . Iye anawononga cuma cake conse koma osapindula kanthu , m’malomwake matendawo ankangokulila - kulila . ” — Maliko 5 : 25 , 26 . Ndiyeno tidzambilana tanthauzo la lotolo . Ummi anavomeleza kuphunzila na Mboni za Yehova m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni . ( Aroma 13 : 1 ) Cifukwa ca ici , nthawi zina anali kupezeka kuti akucilikiza nkhondo m’njila zosiyana - ziyana . Kugwilizana kwambili ndi abale ndi alongo mu mpingo kunathandiza Hannah kuti asaziyewa kunyumba . PANTHAWI ina , Mulungu anadzidziŵikitsa mwa kuchula dzina lake ndi makhalidwe ake kwa Mose . Iwo anaona mnyamata ameneyo ngati katundu wamtengo wapatali kwambili , cakuti anaona kuti akapita naye ku Iguputo adzawapezetsa phindu kwambili . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kudzicepetsa pamene anali kuuza ophunzila ake zocita ? 3 : 15 - 17 . Sindikukumbukila nkhani imene anali kuphunzila , koma ndimakumbukila kuti ana aang’ono anali kutsegula Mabaibulo ao kuti apeze malemba . Unakhulupilika pa zinthu zocepa . Kenako anaona amuna 6 , aliyense wa iwo atanyamula “ cida cake cophwanyila . ” ( a ) Kodi n’ciani cimene timapempha Mulungu kucita tikamapemphela kuti “ Ufumu wanu ubwele ” ? Wiki yotsatila , n’nayambadi kuphunzila na M’bale Hardaker . 2 : 48 ) Ezekieli , kuphatikizapo Ayuda ena amene anali akapolo ku Babulo , ayenela kuti analimbikitsidwa kwambili kuona Yehova akuwacilikiza mwanjila imeneyi . Komabe , dalitso likulu pa zonse , ni mwayi wodziŵa Yehova Mulungu . “ Ndinadziŵana ndi Mike kale kwambili . Akatswili ena aona kuti padzikoli pacitika zinthu zina zikuluzikulu zimene zidzasintha dziko . Koma Satana ndi wodzikonda ndipo sasamala za inu . Koma pamene n’nali kukonzekela kuti nilembe kalata yonena kuti sinidzabwela ku sukulu , panacitika cinthu cina cosaiŵalika . Ena sanacite kufunafuna coonadi , io anacipeza mwina cifukwa cakuti munthu wina anawalalikila . ( Mlal . 3 : 1 , 17 ) N’zomveka kuti tiyenela kuvala mogwilizana ndi nyengo . ( b ) Kodi mungathetse bwanji vuto losamasukila alendo ? Komabe , n’kamodzi mwa zinthu za mtengo wapatali kwa iye . Ndipo lemba la Miyambo 8 : 6 linali ndi mau 20 m’Baibulo lakale , koma tsopano lili ndi mau 13 okha . Tifunika kuvala bwino , kaya tili pa msonkhano kapena poceza cabe . ( b ) N’cifukwa ciani timatha kumvetsa kafotokozedwe komveka bwino ka zinthu zozama ? Khadi la ulaliki linali kapepala kakang’ono kokhala ndi uthenga wacidule ndi wosavuta wa m’Baibulo . Linathandiza ophunzila a Yesu kukhala mbali yaciŵili ya mbeu ya Abulahamu . Yehova adziŵa kuti tifunikila ndalama . Tiziyamikila makhalidwe abwino a akhiristu anzathu na zimene amacita . Koma cifukwa cakuti dziko limasintha malo ake m’cilengedwe pakapita zaka mahandiledi ambili , madeti amene anawagwilizanitsa na zizindikilo zakumwamba sagwilizananso na nthawi pamene dzuŵa likudutsa m’magulu a nyenyezi . Iwo amatengela citsanzo cake cifukwa “ Mulungu ndiye cikondi . ” Tikupemphelelanso kuti muziyenda mogwilizana ndi zimene Yehova amafuna , kuti muzimukondweletsa pa ciliconse , pamene mukupitiliza kubala zipatso m’nchito iliyonse yabwino , ndi kuwonjezela kumudziŵa Mulungu molondola . ” ( Akol . ( Sal . 100 : 3 ) Komabe , kuyambila kalekale , Yehova wakhala akusankha anthu ena , kuti akhale anthu ake apadela . Akafika pamenepa , iye angakwanitse kudzisankhila yekha mabwenzi mwanzelu . Kodi acicepele angalimbikitse bwanji mgwilizano mumpingo na kuthandiza ena kuonetsa kuwala kwawo ? Iye amadziŵa mmene angasamalile zinthu za m’dzikoli ndi kuzigwilitsila nchito bwino . Munthu aliyense padziko lapansi anatengela ucimo umene umatilepheletsa kucita zonse zimene Mulungu amafuna . Kodi mau akuti “ Atate wathu ” amatikumbutsa ciani ? Masiku anonso , makolo ambili acikhristu alimbikitsa ana awo kuyamba utumiki wanthawi zonse ndi kutumikila Mulungu na mtima wawo wonse . Pamene tikambilana njila zinayi zimenezi , zindikilani masitepi amene mufunika kutenga kuti zitheke . Kodi Yehova adzacotsa ciani kuti padziko pakhale mtendele ndi cimwemwe ? Patapita nthawi yocepa , tinakukila m’dela lina labwino kumalile na dziko la Brazil . 3 : 1 - 5 ) Satana ananyoza Yehova ponena za Yobu . ( b ) Tingacite ciani kuti kusinkha - sinkha kwathu kuzikhala kwaphindu ? Kumbukilani kuti kwa zaka zambili - mbili , angelo amene anakhala ku mbali ya Satana anali kutumikila pamaso pa Mulungu . Yehova anali atatsegula khomo kuti pakhale ciwonjezeko pa zisumbu zingapo zimene anthu amakamba Cipwitikizi . Zisumbu zimenezo zinaphatikizapo Azores , Cape Verde , Madeira , ndi São Tomé na Príncipe . Nchito yolalikila imakwanilitsa ulosi wa m’Baibulo . — Maliko 13 : 10 . MMENE BAIBULO LINASINTHILA UMOYO WANGA : Poyamba sindinali kuona ubwino wopanga masinthidwe alionse paumoyo wanga . N’cifukwa ciani Yesu anakamba izi ? Ndimaona kuti ndinacita bwino kwambili kubatizidwa . ” Mwa kuphunzila mipukutu imeneyi , anthu onse , kuphatikizapo oukitsidwa , adzatha kudziŵa zimene Mulungu afuna kuti io acite . 14 - 18 . Komabe , Eunice anatsimikiza mtima kukhalabe okhulupilika kwa Yehova . Kodi mungacule maina a abale ndi alongo amene anakuthandizani pamavuto anu ? Koma mtumwi Paulo anafotokoza zimene zimacitika kwa munthu aliyense amene wadzozedwa . Ganizilani cabe ! Yesu sananyalanyaze vutolo . Kudzikonda kuli ngati dzimbili . M’paradaiso wauzimu ameneyu ni modzala na makhalidwe amene mzimu wa Mulungu umatulutsa . ( Agal . 5 : 22 , 23 ) Ha ! Estienne sindiye anali woyamba kugawa Baibulo kukhala m’mavesi . Conco n’nalandila uphungu ndipo m’kupita kwa nthawi , n’nayambanso kucita bwino mwauzimu . ” N’ciani cidzacitika cifukwa ca kuukila kwa Gogi ? Mfundo yaikulu ndi yakuti : Kukhala ndi zolinga za kuuzimu kudzakucititsani kukonda kwambili zinthu za kuuzimu zimene zidzakuthandizani kukonzekela kudzakhala ndi moyo m’dziko latsopano . ( b ) Ni nthawi iti imene tikuiyembekezela mwacidwi ? Umoyo wa banja lathu unasintha kwambili cifukwa ca mfundo za m’Baibulo , zimene zimafotokoza udindo wanga monga mwamuna ndi tate . Iye ataona anthu amene anali kulila cifukwa ca imfa ya bwenzi lake Lazalo , “ anadzuma povutika mumtima ndi kumva cisoni . ” Amakondana kwambili ndipo amakhala mwamtendele monga banja la pa dziko lonse . A Stephen , amene tawachula kuciyambi kwa nkhani ino anati : “ Tinapwetekedwa mtima kwambili ndi zimene Natalie anacita . Ndipo sitinamvetsetse cifukwa cake anali kukana kuti sanatenge mphete . Koma tinaona kuti anali ndi zaka zocepa ndi nzelu zaumwana . ” Mau a Mulungu amakamba kuti anthu osadziŵa Mulungu angakhale na makhalidwe ena abwino . Satana atagwetsedwa padziko lapansi , io anazunzidwa . ( Chiv . Mwacitsanzo , mwina mumaganizapo kuti kaya mudzakwatila kapena kukwatiwa , ndi kuti mudzakwatilana ndi munthu wotani , ndiponso kuti mudzagwila nchito yotani . Ndiponso pezani malo owala bwino ndi opita kamphepo kabwino kuti mumvetsetse zimene muŵelenga . Kodi Akhristu Ayenela Kukondwelela Khrisimasi ? N’cifukwa ciani Afarisi anali ouma mtima conco ? M’kupita kwa nthawi ndinakhala ndi cidalilo colimba . ” 72 : 1 - 20 . Masiku ano , Satana wapangitsa Akhiristu ena kuganiza kuti angacimwe mmene afunila ndipo Yehova adzapitiliza kuwakhululukila . 14 : 28 ; 17 : 3 ) Kwa nthawi yoyamba , ndinaonanso dzina la Mulungu lakuti Yehova m’Baibulo . — Eks . Sitinasoŵepo cakudya . ” Onani nkhani yakuti “ Cifukwa Cake Kucotsa Munthu Mumpingo Ndi Makonzedwe Acikondi , ” m’magazini ino . Olo zinali conco , iye sanaleke kuwalalikila . Mkristu wofikapo sadziŵa cabe zimene Baibulo limakamba . Ngakhale kuti anali kumva , mitima yao inali youma kwambili . ( b ) Nanga anthu a Yehova masiku ano ali ndi udindo wotani ? Kuwonjezela apo , anthuwo anazindikila kuti ulosi wa pa Salimo 16 : 10 unakwanilitsika pamene Yesu anaukitsidwa kwa akufa . 119 : 35 ) Na imwe mungapeze cimwemwe coculuka poŵelenga Mau a Mulungu . Kodi sizikusangalatsani kumva mau oyamikila amene abale ndi alongo amanena cifukwa ca Nyumba za Ufumu zimene zamangidwa ku madela ao ? Ndipo abale ndi alongo enanso m’madela ambili padziko lonse akusangalala kwambili cifukwa ca Nyumba za Ufumu zimenezi . Nchitoyi ndi ya Yehova . M’dziko latsopano , padzakhala nthawi zina pamene tidzafunika kuonetsa kuleza mtima . Kodi mwaphunzilapo ciani pa citsanzo ca Danieli ? Mwacitsanzo , Yobu anali kudziŵa kuti sangakambe kuti amakonda Mulungu ngati sakomela mtima anthu anzake . Kodi tingacite bwanji zimenezi ? Komabe , anapatula nthawi yophunzitsa ena kuti akhale abusa ndi aphunzitsi . Kodi iye anasintha pamene anakula ? M’bale Knorr anakamba kuti panafunika Baibulo losavuta kuŵelenga ndi kumva monga mmene zolemba za ophunzila a Kristu zinalili . Nayenso mtumwi Paulo anaona kuti kulimbikitsa ena n’kofunika ngako . Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Colinga cokulamulila zimenezi n’cakuti tikhale ndi cikondi cocokela mumtima woyela , m’cikumbumtima cabwino , ndiponso m’cikhulupililo copanda cinyengo . ” 3 : 16 ; 1 Yoh . 4 : 9 ) Ngati Yehova sangacite zimene analonjeza , Mdyelekezi angapeze cifukwa conenela Mulungu kuti ni wabodza , amamana anthu ake zabwino , ndi kuti salamulila mwacilungamo . ( b ) N’ciani cimatithandiza kupitiliza kugwila nchito ya Mulungu ? Kenako anauza Yosefe kuti : “ Popeza kuti Mulungu wakudziŵitsa zonsezi , palibenso munthu wina wozindikila ndi wanzelu ngati iwe . Anthu amene anandilandila anali aulemu ndi okoma mtima . Monga Paulo , Yakobo anafotokoza kuti cikhulupililo ca Mkhiristu woona sicikhala copanda nchito . Kodi m’baleyu anacita ciani ? Cisautso cacikulu cidzafika pacimake pamene maboma onse a m’dzikoli adzawonongedwa , pamodzi ndi onse amene adzakhala kumbali yawo polimbana ndi Ufumu wa Mulungu . ( Yer . Iye wapitilizabe kuonetsa kuti amatikonda mwa kutipatsa zinthu zabwino zocilikiza moyo . ( Mac . 17 : 28 ; Chiv . 16 : 31 ; 20 : 29 ) Levitiko 19 : 32 imati : “ Anthu aimvi uziwagwadila , munthu wacikulile uzim’patsa ulemu ndipo uziopa Mulungu wako . Akatelo , Yehova “ angawalole kulapa , kuti adziŵe coonadi molondola . ” — 2 Tim . KAMBILANANI ZIMENE MALEMBA AMANENA TSAMBA 8 • NYIMBO : 84 , 99 N’naona kuti zocita zawo zinali kugwilizana na zimene Baibo imakamba . Ndimayamikila kwambili Yehova pondithandiza kukhala ndi umoyo wabwino ndi wacimwemwe pakati pa abale a padziko lonse . Iye anakambanso kuti : “ Tsopano nikhulupilila kuti Baibulo imene nili nayo ni mphatso yocokela kwa Mulungu . 15 : 1 ) Tsopano tiyeni tikambilane zinthu ziŵili mwa zinthu zimenezi . Zinthu ziŵilizi ndi kupewa misece ndi kukhala oona mtima m’zinthu zonse . Ngakhale kuti Satana anacititsa Yesu kufa imfa yoŵaŵa , Yesu anakhalabe wokhulupilika kwa Atate wake wakumwamba . Pa Mateyu 5 : 3 pamati : “ Odala ndi anthu amene amazindikila zosoŵa zawo zauzimu , cifukwa ufumu wakumwamba ndi wawo . ” Ngati tikhalabe odzipeleka kwa Mulungu ndi mtima wonse komanso mokhulupilika , ndiye kuti tikum’tumikila ndi mtima wathunthu , ngakhale kuti ndife opanda ungwilo . — 2 Mbiri 19 : 9 . N’ciani cinawathandiza abale na alongo amenewa kuseŵenzetsa mwanzelu ufulu wawo ? 41 : 10 , 13 ) Tikamacita zinthu molimba mtima polambila Yehova , tingakhale na cidalilo cakuti tidzapeza madalitso tsopano ndi mtsogolo . Conco , onse amene amakonda ndi kucilikiza ulamulilo wa Mulungu afunika kucita zimenezi . 2 : 1 , 10 ) Nanga kodi Salimo 16 : 10 imakamba za ndani ? Tikamagwila nchito pamodzi ndi anthu amene timakonda , timayamba kuwakonda kwambili . N’nasainanso fomu ina yofunsila utumiki wa pa Beteli mu 1955 , pa msonkhano wacigawo ku Yankee Stadium , mumzinda wa New York . ( Yer . 25 : 8 - 11 ) Yesaya amene anauzilidwa kulemba kuti Yehova adzabwezeletsa Ayuda m’dziko lao anati : “ Odala ndi anthu onse amene amamuyembekezela . ” Si Mulungu amene amacititsa zinthu zopanda cilungamo zimene timaona . Conco , kaya tidzakhala kumwamba pamodzi ndi Yesu kapena tidzakhala m’paladaiso pano padziko lapansi , zimene zinacitika pa Pentekosite mu 33 C.E . , zimatikhudza . — Onani mau akumapeto . Mawu amenewa mulibe mumpukutu woyambilila wa Baibulo . ( Aroma 12 : 10 ) Mau amenewa aonetsa cikondi camphamvu cimene cili pakati pathu . “ Ndinakhalapo m’Katolika , m’Pulotesitanti , m’Hindu , M’buda wokhala m’nyumba ya ansembe ndipo ndinacita maphunzilo apamwamba a zaumulungu pa yunivesite . Cikondi ca pa abale cimeneci , komanso cikondi cozikidwa pa mfundo za m’Baibulo , cimathandiza anthu a Mulungu kukhala mabwenzi apamtima . Anthu m’dziko lolamulidwa na Satana , alephela kupeza njila zothetsela nkhondo padziko . ( Lev . 16 : 14 , 15 , 19 ) Zocitika zimenezi zinatsegula njila yakuti Yehova akhululukile Aisiraeli macimo ao . 20 : 12 ; Aef . 6 : 2 ) Yesu anagogomezela kufunika kwa lamulo limeneli mwa kudzudzula Afalisi ndi alembi amene sanali kusamalila makolo ao . Iwo anagulitsa nyumba na katundu wawo kuti ndalamazo ziŵathandize pocita utumiki wa nthawi zonse . Mofananamo , tifunika kucitapo kanthu mwamsanga kuti tileke makhalidwe amene Mulungu amadana nawo . Yehova , amene amatiumba , ni wamkulu kuposa woumba wina aliyense . Kuti sanan’thandize , sembe nikali mu ukapolo , mwina n’kanafa . ” Mu 1990 , mwana wathu wina wamwamuna Pavel , amene anali na zaka 19 panthawiyo , anatiuza kuti afuna kukacita upainiya ku cisumbu cochedwa Sakhalin , kumpoto kwa dziko la Japan . Conco , Yehova anali ndi cidalilo cakuti Mwana wake adzakhalabe wokhulupilika akabwela padziko lapansi . Nkhope zawo zinali na makwizi cifukwa ca ukali . Nsembe ya Yesu ndi kuuka kwake zimatsimikizila kuti imfa idzatha . Kodi mumakonda kuŵelenga Baibo kuti mupeze malangizo othandiza ? ( Miyambo 3 : 5 - 7 ) Tikamaphunzila Baibulo ndi kudziŵa mmene Yehova amaonela zinthu , tidzadziŵanso zimene iye afuna kuti ticite pa cocitika ciliconse . Ndiyeno , Yohane anakamba kuti anali kufunila Gayo thanzi labwino monga mmenenso moyo wake wauzimu unalili . Satana anali kudziŵa kuti Yesu anali na ciyembekezo cokakhala mfumu yolamulila mtundu wa anthu . Yehova adzagwilitsila nchito olamulila andale kuononga “ hule ” loipa limeneli . ( Chiv . Kodi makolo anu amafuna kuŵathandiza kuphika ndi kuyeletsa cabe ? ( b ) Kodi dzina lakuti Yesu litanthauzanji ? Nanga iye anacita ciani mogwilizana ndi dzina lake ? Pamene n’nakana , ananipeleka kwa mkulu wa asilikali pa kampuyo . Iye anakamba kuti “ Mwana wa munthu ” adzalekanitsa anthu m’magulu aŵili . ( Yoweli 2 : 28 - 32 ; Machitidwe 2 : 16 - 21 ) Kodi n’ciani cimene cinacitika ? Nanga bwanji ponena za nthawi imene adzalekanitsa nkhosa ndi mbuzi ? ( Agalatiya 5 : 19 - 21 ) Conco , tingadzifunse kuti : ‘ Kodi cikumbumtima canga cimandithandiza kupewa maseŵela amene amalimbikitsa ciwawa , mpikisano , kapena kukonda kwambili dziko langa ? Kufufuza mwa njilayi kwathandiza ophunzila Baibulo oona mtima kukhulupilila kuti Baibulo limene tili nalo masiku ano , ndi Mau ouzilidwa a Yehova . — Yesaya 40 : 8 . Ena angapulinteko nkhani zina pa Webusaiti yathu ndi kupatsako ena amene alibe intaneti , koma mipingo siyenela kucita zimenezi . Mavesi amenewa amati : “ Kunena za Davide mwana wa Jese , iye analamulila Isiraeli yense . Masiku onse amene iye analamulila Isiraeli anakwana zaka 40 . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana makhalidwe ena abwino amene afunika kukhala mbali ya umunthu wathu watsopano . Koma kucita zimenezo n’kofunika kwambili . Yehova ali ngati m’busa wacikondi amene amatsogolela ndi kucenjeza nkhosa zake kuti zisayende m’njila zoipa . — Ŵelengani Yesaya 30 : 20 , 21 . KODI MUNGAYANKHE BWANJI ? Kodi makolo ndi ana ao aakulu angakonzekele bwanji “ masiku oipa ” ? 6 : 10 ; 1 Yoh . 4 : 16 . ( Aroma 8 : 15 , 16 ) Paulo anakamba kuti Akristu odzozedwa ‘ anawakweza ndi kuwakhazika pamodzi m’malo akumwamba mogwilizana ndi Kristu Yesu . ’ Iwo analoŵa mumzinda pa zipata zimene zinasiidwa zosatseka . Ndinapita ku kosi ndipo ndinakhala ndi luso lomenya mbama ndi kuponya zibakela mwa kugwilitsila nchito njila zosiyanasiyana za makalate . Yesu anakula ali na umoyo wacimwemwe . Koma cokondweletsa n’cakuti : Cikondi cikali kuonekela kwambili pamisonkhano yathu . — Yoh . ( 2 Mafumu 3 : 11 ) Mwacionekele , Eliya analimbikitsidwa kwambili kukhala ndi mtumiki wakhama ndi wom’thandiza ameneyu . Mlungu wotsatila , abalewo anakumana pa Nyumba ya Ufumu , ndipo pambuyo popemphela kwa Yehova , anakambilana kwa ola limodzi . Kupatula nthawi yoceza na okalamba n’kolimbikitsa ngako ( Onani palagilafu 11 ) ( Gen . 1 : 28 ) Kodi lamulo limeneli linawaphwanyila ufulu ? Ndiponso pamene Mose ‘ anatambasula dzanja lake kuloza panyanja , ’ Yehova anagaŵa nyanjayo . Mu 1896 , iye analemba kuti : “ Sitifuna kulambilidwa ndi kudzipezela ulemelelo cifukwa ca zofalitsa zathu . Ndiponso banja lina la anthu aciyela linatenga mnyamata wina wacikuda amene analibe kokhala . Kodi tiyenela kupemphela kwa Mulungu kapena kwa Yesu ? ( Ŵelengani Luka 12 : 32 . ) Kumvela malamulo a Yehova na kutsatila mfundo zake kumabweletsa madalitso . Izi n’zimene Salimo 119 : 97 - 100 imakamba . M’nkhani ino , tidzakambilana mmene Mau a Mulungu apitilizila kukhalapo mosasamala kanthu za ( 1 ) kusintha - sintha kwa zinenelo , ( 2 ) kusintha kwa zandale kumene kunakhudza zinenelo , ndi ( 3 ) kuletsedwa kwa nchito yomasulila Baibo . Tsiku lililonse ndimaganizila za Paladaiso . Zinthu zambili zoipa zimene zimacitika masiku ano zimacitidwa na mabungwe osati anthu paokha . Ndipo nzelu zimenezi zimatiteteza ku makhalidwe oipa komanso ku zinthu zina zimene zingatiwononge mwauzimu . Coyamba , amawapezela zinthu zofunika monga cakudya , zovala , ndi malo ogona . Iye anafotokoza cimene cinam’thandiza kusintha maganizo ake . Armen anati : “ Zimene ndinali kuphunzila m’Baibulo ndi kukonda kwanga Yehova zinandithandiza kuti ndileke kukoka . Motelo iye anawauza kuti : “ Ndidzakutumizilani tembelelo ndi kutembelela madalitso anu . ” Ofesi ya nthambi itatsegulidwa ku Mexico City mu 1929 , zinaoneka monga kuti coonadi cidzapita patsogolo . ( Deut . 16 : 16 ) Masiku anonso , kupeleka zopeleka zathu mowoloŵa manja poyamikila na kucilikiza nchito ya gulu la Yehova , ni mbali yofunika kwambili ya kulambila kwathu . Anzathu ena anapatsidwa cilango cogubuduza vimiyala , koma ise tinaliko na mwayi cifukwa sitinapatsidweko cilango cotelo . N’cifukwa ciani ena zimawavuta kukhulupilila kuti Yehova amaŵakonda ? * Kukhomeleza Mau a Mulungu mwa ana anu kumafuna kukhala woleza mtima , koma kuli na mapindu ambili . — Deut . Mabuku onse anatha ndikalibe kufika ku cigawo ca Georgia . ( 1 Akor . 2 : 12 ) Koma tifunika kusamala . Ngakhale zinthu za mu umoyo zimene zioneka monga sizingacititse munthu kugona mwauzimu , zikhoza kutisokoneza kuti tilephele kucita zinthu za kuuzimu . Mtumwi Petulo anatumidwa kupita kunyumba ya Koneliyo , munthu wakunja wosadulidwa . Ali ndi zaka 12 , iye anali pamodzi ndi makolo ake pa msonkhano waukulu . Kodi izi zitanthauza kuti io amamanidwa cakudya copatsa thanzi labwino la kuuzimu ? Mwacidule , n’cifukwa cakuti panali kudzatenga nthawi yaitali kuti lonjezoli likwanilitsidwe . Onani kuti lembali silikamba kuti anthu adzakhala okonda zosangalatsa kuposa Mulungu , ngati kuti Mulunguyo amam’kondako pang’ono . N’kutheka kuti Inoki anayamba kuganiza kuti sadzaonananso ndi a m’banja lake . Akristu oona ali kale paubwenzi ndi Yehova ndipo ali ndi ciyembekezo ca moyo wosatha . Ndiyeno , amagwilitsila nchito cikumbumtima cake cophunzitsidwa bwino kupanga zosankha mwanzelu . Pobwela anali kunyamula nyale zimene zinali kuoneka bwino monga nyenyezi zowala . Satana ananamiza anthu aŵili oyamba kuti Yehova sanafunikile kuwalamulila . Yonatani anakhala bwenzi la Davide ndipo anakhalabe wokhulupilika kwa iye . Ngati mukutumikila Yehova mokhulupilika , mosasamala kanthu za udindo wanu mumpingo , ndiye kuti mukupita patsogolo . ” ( Mateyu 6 : 9 , 10 ) Mu Ufumu wa Mulungu simudzakhalanso nkhondo ya padziko lonse kapena nkhondo ina iliyonse . Pambuyo popempha citsogozo kwa Yehova m’pemphelo , na kumvetsela bwino - bwino pamene mlongo afotokoza nkhawa yake , akulu angam’limbikitse na kum’tonthoza pogwilitsila nchito Mau a Mulungu . — Aroma 15 : 4 . Tisamaganize kuti Mulungu ndi amene akutiyesa . 16 : 3 , 9 . Ngakhale n’conco , Aisiraeli anali ‘ kukayika - kayika . ’ Popeza Yehova anatulutsa Aisiraeli mu Iguputo , io anali ndi udindo waukulu wocitila umboni za ulamulilo wake kwa anthu onse padziko lapansi . 17 Musalole Kuti Cikondi Canu Cizilale M’malo moweluza kapena kukaikila abale ndi alongo athu amene akuvutika , tiyenela kuwatonthoza . ( Yobu 33 : 6 , 7 ; Mat . M’bale ameneyu analinso wodzozedwa ndipo anali wacangu panchito yolalikila . Mwacitsanzo , Mkhristu aliyense amadziŵa kuti ali ndi udindo wolalikila uthenga wabwino . ( Mac . Akandipatsa mabala 4 a sopo , ndinali kutengapo mabala aŵili ndipo ena ndinali kugulitsa . Ndiyeno , dzifunseni kuti , ‘ Kodi zimene chechi yanga imaphunzitsa zigwilizana ndi zimene Baibulo ikamba ? ’ Iye anali kufunsa mafunso amene anacititsa aphunzitsiwo kudabwa kwambili . Nanga njila yabwino yocitila zimenezi ndi iti ? Ngati pambuyo poŵelenga mau amenewa mwaona kuti mumaika zinthu za Ufumu patsogolo , mumadziŵa kuti Yehova akukondwela nanu . Abale athu ambili amalalikila m’magawo amene ali ndi anthu oculuka opanda cidwi , onyoza , kapena ozunza . Kodi Yonatani anali kuwaona bwanji atate ake ? Apun anabwela kudzaticezela patapita miyezi itatu . Sindinayembekezele kuti adzalandila uphungu wanga . * Pakati pa anthu amenewa , pali Mboni za Yehova masauzande oculuka . M’malo mokhumudwa na kapelekedwe ka malangizo , yesetsani kuganizila cifukwa cimene amapelekela malangizo mwanjila imeneyo . Mu kalendala yathu ndi m’kabuku ka Kuphunzila Malemba Tsiku ndi Tsiku , mumapezeka ndandanda ya kuŵelenga Baibulo ya pa nyengo ya Cikumbutso . Koma makolo ake anafunsa kuti , “ Kodi muganiza kuti adzangotilekelela pamene tikucoka ? ” Kapena kukhululukidwa macimo cifukwa ca cikhulupililo canu mu nsembe ya dipo ya Kristu ? Ndipo palibe cinthu cina cokondweletsa kuposa kusonyezedwa ‘ kukoma mtima kwake kosatha . ’ — Yes . Ineyo ndikuthandiza . ’ ” Baibulo limatiuza kuti : “ Iye adzapukuta misozi yonse m’maso mwao , ndipo imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . 5 : 19 ) Mwina palipano tikuvutika ndi ukalamba , matenda , kapena mavuto a zacuma . Gulu la Mboni limeneli limalengeza zimene Mulungu walonjeza kudzacitila anthu mtsogolo . Patangopita nthawi yocepa , tinadadwa kulandila kalata yotipempha kuti tikatumikile ku Portugal . Kodi pamene Rehobowamu anamvela uthenga waciweluzo umenewo anacitanji ? ( Yes . 33 : 22 ) Mbili ya Isiraeli ionetsa zimene zimacitika ngati malamulo olungama a Mulungu atsatilidwa kapena ngati satsatilidwa . Kodi sizingakhale bwino kuti ayembekezeko pang’ono kuti adzabatizike m’tsogolo ? ’ Kodi cikondi capamwamba kwambili n’citi ? 12 : 12 , 17 . Mwacitsanzo , ayenela kuti anaphunzitsidwa na atate wake , a Lameki , amene anali munthu wacikhulupililo . Cifukwa zinapangitsa kuti mgwilizano wathu usokonezeke kwa kanthawi pa zifukwa zosamveka . ” — Julia . Baibo imapeleka zifukwa zotithandiza kukhulupilila kuti Yehova ali na ufulu wolamulila cilengedwe conse . Koma popeza kuti mukuwatayila kumbali ndipo mukudziweluza nokha kukhala osayenela moyo wosatha , ifeyo tikutembenukila kwa anthu a mitundu ina . ya December 8 , 2003 , anakamba kuti : “ Nimayesa - yesa kuti nigonjetse maganizo olakwika . Ayenela kuti anaphunzila za Mulungu mwa kumvetsela kwa acikulile okhulupilika , kwa Mulungu , kapena anali kuŵelenga mipukutu yakale yodalilika . Iye akali “ Yehova mmodzi . ” Zinanithandizanso kuona kuti Akhristu amakondanadi . ▪ Mmene Yehova Amayandikilila kwa Ife Komabe , iye sanali mkazi yekha amene Yesu anali kukonda ndi kulemekeza . N’ciani cingatithandize kuvula umunthu wakale ? M’malomwake zinalimbitsa ubwenzi wake ndi Mulungu . Kodi timatsatila mokhulupilika malangizo atsopano ocokela kwa Yehova ? Ine na amayi tinali kukhala na ambuya ku Burg , tauni ing’ono m’dziko limene kale linali kuchedwa East Germany . 4 : 30 ) Koma cikondi ceni - ceni cimalimbikitsa Mkhristu amene wacita chimo lalikulu kuulula chimolo kwa akulu kuti amupatse thandizo . — Yak . Kwa zaka ziŵili tinali kudalila cabe thandizo la acibale ndi mapisiweki . ( b ) N’cifukwa ciani Yehova anapempha anthu ake kuti ‘ abwelele kwa iye ’ ? Paulo ndi Baranaba atacoka ku Derbe , “ anabwelela ku Lusitara , ku Ikoniyo ndi ku Antiokeya . Ganizilani citsanzo ca Takuya , * amene anali kulimbana ndi cizolowezi cotamba zamalisece ndi kuseŵeletsa malisece . Conco , kuti tithaŵile kwa Yehova , tiyenela kukhulupilila nsembe ya Yesu . Posacedwa , padzikoli padzakhala anthu okhawo amene asankha kukhala kumbali ya ulamulilo wa Yehova . Kodi muona kuti n’zotheka anthu kupanga boma lotelo ? — Ŵelengani Yeremiya 10 : 23 . Ndiyeno , tinauyamba ulendo wa panyanja kupitila ku Rotterdam , ku nyanja ya Mediterranean , ya Suez , ya Indian , ku Malaysia , mpaka ku Hong Kong . Masiku 47 tili panyanja ! Mulalikila kwambili masiku ano . ’ ” Limalekelatu kugwilila njingayo ngati mwanayo wadziŵa kuyendetsa . ( Miyambo 31 : 15 ; Mateyu 24 : 41 ) M’nthawi zakale , anthu ambili anali kulima tiligu wocedwa emmer . Ngakhale n’conco , apeza madalitso ambili poyelekezela na zimene ataya . — Ŵelengani Maliko 10 : 29 , 30 . Motani ? M’caka ca 1891 , katswili wina wa Ciheberi dzina lake Franz Delitzsch analemba kuti : “ Baibo ya Ciheberi imene anamasulila inali ndi mau ambili amene Akhristu sanali kuwaseŵenzetsa , ndipo ikali yothandiza pofufuza zinthu . Iye anali kuonetsetsa kuti wasankha mau oyenelela . ” Mungapeleke ndalama , ndolo ( masikiyo ) , mphete , zibangili , ndi zinthu zina zamtengo wapatali . ( a ) Kodi nkhani ya Naboti timaimvetsetsa bwanji masiku ano ? Nanga citsanzo cake ndi cothandiza bwanji ? N’cifukwa ciani timalakwitsa ? Kodi cofunika n’ciani pa lililonse la masitepu amenewa ? Nanga inu ndinu ndani ? N’naphunzila kuseŵenzetsa mendo pocita zinthu . Kusinkhasinkha pa zinthu zabwino zimene Yehova waticitila kudzatithandiza kuyamikila kwambili cikondi cake cosatha . — Ŵelengani Salimo 77 : 11 , 12 . DZIKO : MEXICO Zoonadi , Mulungu anacititsa Bezaleli ndi Oholiabu kukhala ndi luso lofunika kuti akwanitse kugwila nchito yonse imene anawapatsa . — Eks . ( Luka 18 : 29 , 30 ) Njila ina yaikulu imene Yehova adzaonetsela kukoma mtima kwake kwakukulu padziko lapansi , ni mwa kuukitsa anthu “ m’Manda . ” N’naona kuti n’nali n’zolinga zabwino , ndi kuti tsogolo langa linali lowala . Timaŵelengamo nkhani zambili pamene Mulungu anadalitsila atumiki ake okhulupilika . 2 : 44 ; Chiv . ( Yuda 7 ) Ocita zosangalatsa amapangitsa anthu kuona khalidwe la ciwelewele monga labwino , lopanda zotulukapo zilizonse zoipa . Conco , kukhululukidwa kwathu macimo na kupatsidwa ciyembekezo codzakhala na moyo kwamuyaya , cilidi cisomo cabe ca Mulungu . Ndiyeno , Elisa anafika pamodzi na amake a mwanayo . — 2 Maf . Kupsa mtima kungayambitse matenda monga a BP , a m’mimba , ndi a m’cifuwa . Nkhawa m’banja imawonjezekanso pamene mkazi wakhala na pakati . Cimatiŵaŵa kwambili tikamvela nkhanza zimene anthuwo amacitila ana , okalamba , ndi anthu ena ovutika . Tidziŵa zimenezi cifukwa Yuda , amene anali m’bale wake wa Yesu , anauzilidwa kulemba ulosi wa Inoki zaka zambili pambuyo pake . ( Yes . 33 : 24 ; 35 : 5 , 6 ; Chiv . Ndiyeno Eliya anauza mtumiki wake wophunzitsidwa bwino ameneyu kuti aleke kumutsatila , koma Elisa anamuuza katatu konse kuti : “ Sindikusiyani . ” Pamwamba pa mapuwo pali kapikica koonetsa paradaiso . Lonjezo limeneli linadabwitsa Baraki . 5 : 11 - 13 ) Akalibe kubwezedwa mu mpingo , afunika coyamba aonetse ‘ zipatso zosonyeza kuti walapadi . ’ ( Luka 3 : 8 ; 2 Akor . 1 : 17 ) Moyo wathu ndi mphatso ya mtengo wapatali yocokela kwa Yehova . Yehova akudalitse cifukwa ca zimene wacita . ” — Rute 2 : 8 - 12 . Ndipo munaphunzitsidwa kuti mukhale atsopano mu mphamvu yoyendetsa maganizo anu , ndi kuvala umunthu watsopano umene unalengedwa mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu ndipo umatsatila zofunika pa cilungamo ceniceni ndi pa kukhulupilika . ” Yesu mokondwela anagwila nchito imene Yehova anam’patsa pamene anali padziko lapansi monga munthu wangwilo . Kodi mpingo ungatonthoze bwanji anthu amene ali na cisoni ? Iwo anati : “ Timathandizila ana athu kuona cikondi ca Yehova ndi kutiganizila kwake pa zonse zimene anatipatsa . ” Iye analiko pasanakhale anthu , angelo ndi Mwana wake wobadwa yekha . Kutangwanika na kulema : Atumiki a Yehova amakhala otangwanika nthawi zambili . Conco , mu 1967 , ndinaleka nchito yovina , ndipo ndinayamba kugwila nchito pa famu ina yaikulu pafupi ndi makolo anga . 1 : 17 ; Chiv . 4 : 11 ) Kumbukilani mau ocititsa cidwi amene Mfumu Davide inakamba ponena za udindo wapamwamba ndi wapadela wa Yehova . * Mwacitsanzo , ena amakaikila ngati kacala kothela ka ku miyendo kali ndi nchito iliyonse . Conco , zinali zovuta kuti atsike kukapempha mpeni wina . Mau ena amene anthu amakamba amene amatanthauza mauthenga osoceletsa ndi monga akuti ‘ mabodza , cinyengo , ndi kupusitsa . ’ — Propaganda and Persuasion . Koma Luka analemba kuti : “ Yosefe , mwana wa Heli . ” ( Mat . 24 : 45 ) Ngakhale m’zaka zoyambilila zimenezo , kagulu kocepa ka abale odzozedwa amene anali kutumikila ku likulu ku Brooklyn , New York , kanali kukonza ndi kupeleka cakudya cauzimu kwa otsatila a Yesu . “ CIMENE MULUNGU WACIMANGA PAMODZI . ” Monga mmene taonela , m’Baibo muli nkhani zambili zoonetsa mapindu amene tingapeze tikakhala odziletsa ndi mavuto amene tingakumane nawo cifukwa ca kusadziletsa . Kuphonya pa kamvedwe ka zinthu zauzimu n’koopsa ngako . Iye wavala citambala kumutu Yelekezelani kuti ndinu Asa . Mofanana ndi Aisiraeli , ifenso tingasiye kukhala oyamikila , ndipo tingayambe kuona ubwenzi wathu wamtengo wapatali ndi Yehova kukhala wosafunika . Tingasiyenso kuyamikila zinthu zabwino zimene Yehova waticitila . — Sal . Koma kwa anthu a Cichainizi ndi buku lacilendo ndipo n’losathandiza . ” ​ — LIN , CHINA . M’nthawi za Yesu , amalonda ena anali kuyenda mpaka kufika ku nyanja ya Indian n’colinga cokapeza ngale zamtengo wapatali . Ndipo nkhani yokhudza ulamulilo wa Mulungu siinathe . Tikamatsutsa Satana timakhala adani ake , ndiponso adani a onse amene ali kumbali yake pa nkhani ya ulamulilo wa cilengedwe conse . Pamene mtumwi Paulo anapita kukacezela abale ake ku Roma , io anayamikila cifukwa ‘ analimbikitsana . ’ Mnzanu wa m’cikwati akakulakwilani , pewani kukaikila zolinga zake . Nditafika zaka 12 , ndinayamba kucita mwambo wa mapemphelo a Asilamu , umene umacitika kasanu patsiku , wochedwa namazi . 11 : 24 - 27 ) Kukamba zoona , kungakhale kupanda nzelu kuyamba kuganiza kuti ‘ tinataya mwayi . ’ Tsiku lina madzulo atanyamula madzi mu mtsuko wake , mwamuna wina wacikulile anathamanga kudzakumana naye . N’nakondwela kwambili nitaphunzila kuti moto wa helo si ciphunzitso ca m’Baibulo . Ambili a ife timakumana ndi zinthu zopanda cilungamo m’dziko lino loipa . Cikumbutso ca mu 2014 cidzacitika pa Mande , April 14 dzuŵa litaloŵa . Nanga timacita bwanji munthu wina akakamba mau osinjilila mbali zina za cikhalidwe ca kwathu ? 20 : 8 - 13 ; 2 Mbiri 32 : 24 ) Pa nthawiyo , Mulungu anamusiya Hezeziya , ndipo iye anaonetsa Ababulo “ zonse za m’nyumba yake yosungilamo cuma . ” TENGELANI CIKHULUPILILO CAWO | DAVIDE ( Ŵelengani Zekariya 2 : 8 . ) Ambili mwa abale odzozedwa amene n’nali kutumikila nawo anatsiliza moyo wawo wa padziko lapansi . Koma mu 33 C.E , Yesu Khristu anakamba motsimikiza kuti Yerusalemu adzaonongedwa . Popeza imfa inafika kudzela mwa munthu mmodzi , kuuka kwa akufa kunafikanso kudzela mwa munthu mmodzi . Anthu akumeneko ayenela kuti anali kumva cinenelo ca Cigiriki , koma anali kukamba Cilukaoniya cimene cinali cinenelo cao . Olo kuti M’bale Russell ndiye anali kukamba nkhani kaŵili - kaŵili , anazindikila kuti “ Gulu la Mulungu silidalila munthu mmodzi ” cifukwa “ iyi si nchito ya munthu , koma ya Mulungu . ” M’nkhani yotsatila tidzaphunzila mmene kutsatila Khalidwe Lopambana kungatithandizile mu ulaliki . [ Mau apansi ] Koma bwanji ngati mavuto amene mukumana nawo sakutha mwamsanga ? Kodi nidzakhala m’ndende kwa nthawi yaitali bwanji ? ’ Dziko la Satana lidzaonongedwa , koma gulu la Yehova padziko lapansi lidzapulumuka . CIFUKWA CAKE GULU LA YEHOVA LIKUPITABE PATSOGOLO Monga mmene Baibulo limanenela , ana amapindula ngati makolo amakhala nao ndi kuwaphunzitsa . — Miy . Kuyankha Mafunso a m’Baibulo Kodi Baibulo ndi Maudi a Mulungu ? Lemba la Genesis 17 : 7 limanena kuti lidzakhala “ pangano mpaka kalekale . ” Kuti tipewe kucenjenekewa na zinthu zakuthupi ndi kuonetsa kuti timakondadi Khristu , tifunika kupitiliza kuika zinthu zauzimu patsogolo . Tikatelo , ndiye kuti tasankha “ cinthu cabwino kwambili . ” “ Anamwali anzake ” a mkwatibwi wa Kristu adzasangalala kwambili akadzaona madalitso amene cikwati ca Mwanawankhosa cidzabweletsa m’dziko latsopano . N’zoonekelatu kuti Yosefe sanali kudziŵa yankho lake , koma n’zosakaikitsa kuti iye anali kupemphela kwa Mulungu za nkhaniyi . Paulo anati : “ Muzitsanzila Mulungu , monga ana ake okondedwa , ndipo yendanibe m’cikondi , monganso Khristu anakukondani n’kudzipeleka yekha cifukwa ca inu . ” ( Aef . Iwo amapatula nthawi yolalikila anthu pa masitesheni a basi ndi a sitima , m’mamaketi , m’mapaki ndi pamene pamapitila anthu ambili . ( Genesis 3 :⁠ 3 ) Komabe iye sakakamiza anthu kuti azimumvela , m’malo mwake amawalimbikitsa kucita zabwino kuti apindule . ​ — Ŵelengani Yesaya 48 : ​ 18 , 19 . Onani mmene umbombo wa Akani unakulila msinkhu . Komabe , patapita zaka pafupifupi 1,200 , William Tyndale anayamba kumasulila Baibulo m’Cingelezi . Tithandizeni Yehova Mulungu wathu cifukwa tikudalila inu , ndipo tabwela m’dzina lanu kudzamenyana ndi khamuli . Kenako , iye anawauzanso kuti : “ Tsopano opani Yehova ndi kum’tumikila mosalakwitsa ndiponso mokhulupilika . ” Mose anakamba mau amenewa pamene anali kukamba nkhani yake yotsiliza ku mtundu wa Aisiraeli . ( a ) Mogwilizana ndi Yohane 3 : 16 , kodi Mulungu anacitanji kuti apulumutse anthu ? Yehova anali kum’konda Mariya ndi kum’khulupilila . Ndiye cifukwa cake anamupatsa mwai wapadela umenewu . Zikumbutso zimenezo zimatilimbikitsa kukhala otangwanika mu utumiki wa Mulungu , ndiponso zimatithandiza kudziŵa kuti cizindikilo ca kukhalapo kwa Kristu cikukwanilitsidwa . Ngakhale kuti takhala tikupempha thandizo kwa nthawi yaitali , sitiyenela kuleka kupempha . ( Aroma 5 : 8 ) Cifukwa cakuti mphatsoyi inapelekedwa “ pamene tinali ocimwa , ” dipo imationetsa mmene Mulungu amatikondela olo kuti ndife ocimwa . Timagwilitsilanso nchito njila zina za mayendedwe . Harold Camping , amene amalosela za kuonongedwa kwa dziko , analengeza pamodzi ndi ophunzila ake kuti dziko lapansi lidzaonongedwa mu 2011 . ( b ) Ndi mafunso ati amene acinyamata ayenela kudzifunsa ? Pasanapite nthawi , Yehova anathetsa ciletso cimene cinali copinga cacikulu ngati phili , ndipo nchito yomanga kacisi inatha mu 515 B.C.E . ( Ezara 6 : 22 ; Zek . Limenelo linali tsiku lakuti Gary abatizike . Alonso anakamba kuti : “ Cifukwa cogwilitsila nchito mankhwalawo , n’nakhala kawalala komanso n’nayamba kugulitsa mankhwala osokoneza ubongo . 9 Kodi Mumalola Kuti Woumba Wamkulu Akuumbeni ? Nthawi zonse Abulahamu akayang’ana nyenyezi kumwamba , anali kukumbukila lonjezo la Yehova lakuti adzaculukitsa mbeu yake . Kodi sizokondweletsa kudziŵa kuti Mulungu afuna kuti tikhale ndi umoyo wabwino ? Kulephela kuseŵenzetsa bwino ufulu kwa Adamu kunabweletsa mavuto osaneneka kwa mbadwa zake mpaka lelo . Kodi zinali zotheka kuti Aisiraeli adzamasukanso ndi kukalambila Mulungu mwaufulu ? Pamene mtumwi Paulo anafika pa doko la ku Potiyolo , ananyamuka ulendo wake wopita ku Roma . Atayandikila ku Roma , Akhristu a kumeneko anabwela kuti amulandile . ( Deut . 30 : 19 , 20 ; Yos . Msulami anali ngati mundawo cifukwa anali kukonda cabe m’busa . Kodi amuna okhulupilika akale amene anali na luso lotsogolela anthu ndiwo adzayambile kuuka kuti azikatsogolela anthu a Mulungu m’dziko latsopano ? “ Cikondi , cimwemwe , mtendele . ” Zinali zokopa koma zinali zoipa , ndipo zinanicititsa kuti nizidziimba mlandu . Kodi mungayelekezele kuti mukusangalala ndi madalitso amene Mulungu walonjeza ? Tinakhalanso na mwayi wodzalandila moyo wosatha . — Ŵelengani 1 Yohane 4 : 9 , 10 . Tifunika Kukhala Oyela m’Makhalidwe Athu Onse , 11 / 15 Mwina ena amakusekeni kapena kukunyozani kusukulu cifukwa cokana kucita zinthu zina monga Mboni ya Yehova . 16 Akristu onse amene ali ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi amathandiza odzozedwa kugwila nchito yolalikila za Ufumu . Mkristu aliyense anafunikila kucita khama kuti akhale wolimba kuuzimu . Ndi mmene timacitila bwenzi lathu likatipatsa mphatso yabwino . Timayesetsa kuigwilitsila nchito bwino . Iye anati : “ Masiku ano anthu safuna kugwila nchito tsiku lonse kuti apeze zofunikila pa umoyo . ” Ine ndi Loraini tili mu ulaliki ku Fiji ( Luka 6 : 36 ) Koma sikuti Yehova adzapitiliza kucitila cifundo anthu oipa mpaka kale - kale . Apa Yesu anali kuthandiza ophunzila ake kuzindikila kuti nkhawa zosayenela kapena zopitilila malile sizithandiza . Nchito zimenezi zimaphatikizapo zimene mumacita pampingo , monga kupita kumisonkhano ndi kulalikila . Komabe , anali na cikhulupililo cakuti Yehova , amene analenga anthu , sangalephele kumukumbukila na kumuukitsa . Buku Losavuta Kumvetsetsa 4 Cifunilo cimeneco n’cakuti akhale ndi banja la ana akuuzimu ndi aumunthu odzipeleka kwa iye . Makonzedwe amenewo anakhazikitsidwa mu 29 C.E . pa ubatizo wa Yesu pamene iye anadzozedwa kukhala Mkulu wa Ansembe pa kacisi wamkulu wauzimu wa Yehova . — Aheb . ( Ŵelengani Yesaya 30 : 20 , 21 . ) ( Genesis 5 : 24 ) Kodi Mulungu anatenga Inoki m’njila yabwanji ? Kenako anawafunsa kuti : “ Nanga inu sindinu amtengo wapatali kuposa mbalame kodi ? ” Ngakhale kuti abululu ake na anzake anam’limbikitsa kuti atumize mwana wake kwa makolo ake , iye anaona kuti kucita zimenezo n’kosayenela . Anthu amaganiza kuti m’nyumba zimenezi ndi mmene anthu anali kugona ndiponso kudziyeletsa asanaloŵe m’kacisi . “ Mwana Wanga Wokondedwa ndi Wokhulupilika mwa Ambuye ” 12 N’cifukwa ninji tiyenela kukonda Yehova ? Ningacite ciani kuti banja langa likhale lacimwemwe ? Nanga n’cifukwa ciani masiku ano tifunika kutsatila citsanzo cake ? Panthawiyo ndinali kukonzekela mayeso a kusukulu . Conco , kwa miyezi itatu ndinacita zimene makolo anga anali kufuna . Tinayesetsa kuphunzitsa ana athu kuti azikonda Yehova na kum’tumikila . Pamene tiganizila mozama za masomphenya a Zekariya , timadziŵa kuti ndise otetezeka mu mthunzi wa mapili aŵili ophiphilitsa . Buku ya The International Standard Bible Encyclopedia inati : “ Jerome anafuna kukonzanso mau ena amene sanamasulidwe bwino , kukonza zimene zinalakwika , kucotsamo mau ena osafunika amene anawonjezelamo , na kubwezeletsa mau ena amene anacotsedwamo . ” ( 1 Yoh . 5 : 14 ) Conco , tiyenela kuthandiza anthu kudziŵa kuti pemphelo silimatithandiza cabe kuti timveleko bwino , koma ni njila yabwino imene timafikila ku “ mpando wacifumu wa kukoma mtima kwakukulu . ” ( Aheb . Iwo anali na cikhulupililo colimba , ndipo anakhalabe acimwemwe ngakhale kuti anakumana na mavuto . Tikakhala m’boti tinali kuona nsomba zochedwa madolofini zikuseŵela pamadzi . Ndipo tinali kungomva congo ca boti tikamayenda pa madzi . Katswili wina wa sayansi wacigiriki dzina lake Aristotle , wa m’zaka za m’ma 300 B.C.E . , anali kuphunzitsa kuti zinthu zimene zimawonongeka ni za padziko cabe , koma zinthu za ku thambo sizisintha kapena kuwonongeka . Riana anakamba kuti : “ N’naona kuti Yehova ananithandiza pa nthawi imene n’nali kufunikadi thandizo . Munthu amene anam’patsa moni anali mnzake amene anali kuphunzila naye kusukulu . Onse sanatumikilepo Yehova . N’nayopa kwambili koma n’nacita cidwi na zimene Atate anacita . 5 : 28 , 29 ) Conco , kudzikonda pa mlingo woyenelela n’kwabwino . Ndiye cifukwa cake , ngati mwafufuza m’Baibo , simudzapezamo vesi imene pali mau akuti “ mzimu wosafa . ” Anthu ambili pa nthawiyo anali a ciwawa ndi a ciwelewele . Izi zikanacititsa kuti iye afooke . Yehova amaona mitima , ndipo amadziŵa kukhulupilika kwa anthu ake . Ngakhale kuti anthu ambili alibe cikhulupililo mwa Mulungu , Mau ake afalitsidwa kwambili kuposa buku lililonse m’mbili yonse ya anthu . Tsiku lililonse tinali kupemphela ndi kudalila Yehova . Nthawi zina , tinali kudya cabe mango za m’mitengo imene tinali kupeza m’njila . ” — Afil . Analembelanso kalata nthambi ya ku Canada ndi ya ku Ghana . 73 : 16 , 17 ) Inunso ngati mulambila Yehova mokhulupilika , mungakhale na maganizo oyenela . Colinga canu cotumikila Mulungu cingakhudzenso zosankha zanu ponena za cikwati ndi nchito . Kodi pazocitika zimenezo malangizo a m’Baibulo akuti tiyenela ‘ kukhulupilila Yehova ’ ndi osathandiza ? ( Miy . ( Agalatiya 5 : 22 , 23 ) Ndipo mungaphunzile zimene simuyenela kucita ulendo wotsatila . ( Aheb . 9 : 12 ) Mphatso imeneyi siizatha nchito olo pang’ono , ndipo palibe angatilande . Iye anati : “ Nimayesetsa kukhala womasuka na ena . 11 : 1 - 9 . Cifukwa cokhala kutali ndi Jimmy , Marilyn anayesa kulimbitsa cikondi cao mwa kum’tumizila ndalama ndi mphatso . Ndiponso sipadzakhala kusonkhetsa ndalama . Ngati umboni ulipo , zingatipatse cifukwa cina cokhalila na ciyembekezo monga ca Marita , cakuti akufa adzauka . Tsopano , Delphine anamvetsa kuti mau awa ndi oona , akuti : “ Masiku a moyo wathu amangokwana zaka 70 , ndipo ngati tili ndi mphamvu yapadela amakwana zaka 80 . Mwa mau na zocita zake , Yesu anaonetsa kuti Cilamulo ca Mulungu ni cangwilo , copindulitsa , ndiponso kuti zonse zolembedwa m’cilamuloco sizingalephele kukwanilitsidwa . — Mat . Makambilano ena anali opindulitsa kwambili , ndipo ambili anatenga mabuku athu ndi magazini . C.E . , asayansi anayamba kukhulupilila kuti nyenyezi na mapulaneti onse , zioneka kuti zinangolenjekeka m’malele . Ngakhale kuti simungadziŵe zimene zili m’mitima ya anthu , nanunso mungakhale ndi luso lozindikila . Ndiyeno , ndinatumikila monga mpainiya kwa zaka 5 . Yehova satikakamiza kuti tizicita zimene amafuna . Aisiraeli anagwapo pa nchito imeneyo . Cifukwa cakuti Baibo imatilangiza kuti tiyenela kutengela citsanzo ca Yehova . 13 : 1 - 10 . Eya , ngati muonetsa cikondi kwa abale na kuwalemekeza , mudzapewa zinthu zobweletsa nkhawa . — Aroma 12 : 10 . Tikatelo , io sangafunikile kusiya banja lao ndi kupita kukagwila nchito ku dela lina . — Miy . 3 : 1 - 27 . Umenewu ni mtendele wa m’maganizo umene umatiteteza ku nkhawa za paumoyo . Monyoza anati , ‘ Yehova wako ali kuti ? ’ ” Mwacitsanzo , pamene kunali nkhondo ku Balkans , makolo ambili acikristu sanali kugwila nchito . Izi zinacititsa kuti makolo azikhala panyumba nthawi yaitali . Iwo anali kuphunzila pa sukulu ya anthu ogontha imene ine n’nali kuphunzilapo . Kodi Mau a Mulungu angatithandize bwanji kupewa maganizo oipa ? ( 2 Tim . 3 : 14 , 15 ) Ndithudi , pali umboni wokwanila wotsimikizila kuti njila imene Yehova wakhala akugwilitsila nchito kwa zaka pafupi - fupi 100 potiphunzitsa coonadi , ni yodalilika . — Mat . Kukwela pamwamba pa phili kudzakuthandizani kuti mukhale pamalo otetezeka . Anthu oipa , mabungwe acinyengo , ndi makhalidwe oipa zabweletsa mavuto ambili padziko lapansi . Kodi mudziŵako njila ina iliyonse yothandiza kuti uthenga wabwino wa Ufumu ufalikile padziko lonse lapansi ? M’kalata yake yaciŵili yopita ku Akorinto , Paulo anafotokoza mtima umene tiyenela kukhala nao popatsa zinthu anthu ena . Kodi mumagwilitsila nchito zimene mumaphunzila ? Cifukwa nchito yolalikila anali kuikonda . Khama ndi lofunika kuti tikhalabe oyamikila kwa Yehova . Coyamba , tiyenela kuzindikila zinthu zabwino zimene Yehova waticitila . Ndiyeno , tiyenela kuona mmene zinthu zimenezi zimasonyezela cikondi cacikulu cimene Mulungu ali naco pa ife . N’nali kuopa kucoka kwathu n’kusiya umoyo umene n’nazoloŵela , komanso kusiya acibululu , mpingo , na nyumba yathu . Kodi zokamba zathu na makhalidwe athu zingapindulitse bwanji anthu ena mwauzimu ? Mofananamo , makolo angacite cimodzimodzi ndi ana anu . Nchito yolalikila komanso zotsatilapo zake zabwino ndi mbali ya cizindikilo cimene Yesu anapeleka cosonyeza kuti tikukhala m’nthawi ya mapeto . GULU LA AKRISTU LINAKHAZIKITSIDWA M’NTHAWI YA ATUMWI Kodi Yesu anawauza ciani atsogoleli acipembedzo aciyuda a m’nthawi yake ? Tiyeni tipite kukakwela phili la Yehova . . . Kukhala ndi cithunzi m’maganizo mwathu ca mphoto ya mtsogolo kudzatithandiza kupilila . Sitima yapamadzi ya Lusitania inamizidwa mu May , 1915 , ku gombe la kum’mwela kwa dziko la Ireland . Mwacionekele , nthawi zambili mumakamba mau amenewa popatsa ena moni . Olo n’conco , iwo safunika kusiyila ena udindo wawo wophunzitsa ana . ( b ) N’cifukwa ciani Davide anam’dela nkhawa Solomo ? Nimapezabe cimwemwe mwa kucita maulendo aubusa Ngati tithandiza ena , timakhala acimwemwe , odekha , ndi acikondi , ndipo timakhala Akristu okhwima . ( Aef . Koma zimene anthu opanda ungwilo angacite , sizingacititse kuti uthenga wabwino ‘ ukhazikitsidwe mwalamulo ’ pa mlingo wokwanila . Phili linalo liimila Ufumu wa Mesiya wolamulidwa na Yesu . ( Dan . * Imeneyi yakhala mphatso yabwino kwa anthu amene amavutika kuŵelenga kapena kumvetsetsa cingelezi . Nthawi zambili , zopeleka zimapelekedwa mwamseli . N’cifukwa ciani Mulungu anam’sankha kukhala mai wa Yesu ? Koposa zonse , moyo wao unadalila pa ubale wao ndi Mpatsi Wamoyo . ( Deut . Yehova ndi Yesu anathandiza Petulo kuthetsa cikaikilo ndi mantha . Mwacidule , Yesu amafuna kuti tizimumvela . Nsomba , ndasiya kukhala wa Mboni za Yehova ndi colinga cakuti ndimasulidwe . ” Tsiku loyamba kupita mu utumiki , iye ananipempha kuti , ‘ Kodi munganithandizeko kuphunzitsa maphunzilo anga a Baibulo ? ’ 1 / 1 Zimene Mulungu Wakucitilani , 3 / 1 ( Vesi 11 ) Zimenezi zinali kudzacitikila mtundu wa Isiraeli ndiponso “ Isiraeli wa Mulungu , ” amene ndi Akristu odzozedwa . Titabwelela ku Graz , n’nayamba kupezeka pa misonkhano yonse . Iwo ayenela kuti anawatuma kuti akamve za cizindikiloco . ( 2 Maf . Iyayi . Nsembe Yopseleza : Nsembe yopseleza imachulidwa m’Cilamulo ca Mose . ( Isa . 60 : 22 ) Anthu amene amagwilizana ndi gulu limeneli ndi otetezeka mwakuuzimu . ( Miy . Komanso n’kutheka kuti munthu wina anatikhumudwitsa m’mbuyomo , koma tikulephela kuiŵalako colakwaco . Cikondi cangwilo ca Mulungu na cilungamo cake , zinamusonkhezela kuti atimasule kuukapolo wa ucimo na imfa umene tinatengela . Iye anati : “ Tsiku lina , n’nali kucititsa msonkhano wa mpingo , koma sin’nali kumvetsetsa zimene abale na alongo anali kuyankha . Timafunika “ kumenya mwamphamvu nkhondo yacikhulupililo . ” Iye anakamba kuti : “ Ndinaphunzila nchito zosiyanasiyana kotelo kuti ngati nchito ina yasoŵa ndizitha kugwila ina . ” Afunikanso kutamandidwa cifukwa ca cikondi cake kwa anthu , cimene anacionetsa mwa kutumiza Mwana wake monga nsembe ya dipo . Coyamba , ganizilani mmene Yehova wakuthandizilani . Akuseŵenzetsa kapepa kauthenga kakuti Kodi Baibo Mumaiona Bwanji ? N’zokondweletsa kwambili kutumikila pamodzi na abale athu ku Philippines . * Iye anadzipeleka ndithu kwa Mulungu . Kaciŵili , patatsala pafupi - fupi caka cimodzi kuti Yesu aphedwe , ophunzila ake atatu anamva Yehova akukamba za Yesu kuti : “ Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa , amene ndikukondwela naye , muzimumvela . ” Limati : “ Dziko la pa nthawiyo linaonongedwa pamene linamizidwa ndi madzi . Conco , m’nkhani ino tidzakambilana mafunso atatu awa : Kodi makonzedwe a mizinda yothaŵilako aonetsa bwanji cifundo ca Yehova ? Zikakhala conco , iye angafunike kuononga nthawi ndi ndalama zambili kuti akonze galimotoyo . Komabe , lemba la 2 Timoteyo 3 : 4 limakamba za kukonda zosangalatsa koiŵala nako Mulungu . Kodi Satana amaseŵenzetsa ciani pofuna kusoceletsa anthu ? Nanga adzabwela bwanji ? Ena amati palibe vesi lina limene limafotokoza mwacidule ndi momveka bwino cikondi ca Mulungu pa anthu ndi njila yowapulumutsila . N’cifukwa ciani Mdyelekezi amafuna kutilefula ? ( b ) Kodi makolo angathandize bwanji ana awo kuti azitengako mbali pa misonkhano ? Ena poyamba amavutika maganizo , koma amapilila ndipo amayamba kumvelako bwino . Iye anakonza zakuti awombole mbadwa za anthu aŵili opandukawo , podziŵa kuti ena mwa ana awo adzayamikila cikondi cake . ( Gen . 3 : 15 ; 1 Yoh . Kodi Hezekiya anaonetsa bwanji kuti anadalila Mulungu ndi mtima wonse ? Aisiraeli anali kuliza lipenga pofuna kupeleka uthenga . Comalizila , taona mmene kukhala na “ maganizo a Khristu ” kungatithandizile kukhala munthu wauzimu . Tsopano tiyeni tikambilane zitsanzo zingapo za m’Baibulo zimene zingatithandize kuona kufunika kokhala ogwilizana . Koma m’malo molandila uphungu , Sauli anapeleka zifukwa zodzikhululukila , kukankhila ena mlanduwo , ndi kucepetsa colakwa cake . ( 1 Sam . * — Mlal . Mwadzidzidzi , Yesu anaonekela ndi kuyamba kuyendela nao limodzi . Kodi abale ndi alongo ena ananena ciani poyamikila Nyumba ya Ufumu yatsopano ? N’cianinso cingakuthandizeni kukhala osangalala ndi kupindula pamene mukali mbeta ? Koma popeza ndinali kugwila nchito mu hotelo maola 72 mlungu uliwonse , coyamba ndinafunika kusintha zinthu zina . Pocita ulaliki wa kunyumba ndi nyumba , timagwilitsila nchito pempheloli pofuna kuthandiza eninyumba kumvetsa kuti Ufumu wa Mulungu ndi boma lenileni limene lidzasintha zinthu pa dziko lapansi . Tili ndi cidalilo cakuti Yehova adzadalitsa kuyesayesa kwanu kuti muzilalikila anthu a m’gawo lanu panthawi yoyenela . N’cimodzi - modzi na gulu la Yehova . ( Aef . 4 : 26 , 27 ) Kukamba kuti “ pepani nakukhumudwitsani , ” kumafuna kudzicepetsa na kulimba mtima . Mwina zimene angakuuzeni zingakuthandizeni kuganizilanso zolinga zanu . Patapita nthawi , ophunzilawo anatengela citsanzo cake ca kudzicepetsa . — Machitidwe 3 : 12 , 13 , 16 . 4 : 8 . Lekani ndingosiila ena nchitoyi . ’ Iye anati : “ Nthawi zambili , nimaona ngati kuti Yehova ali nane patali ndipo safuna kukhala Mnzanga . ” 20 Kodi Mumaona Kufunika Kopita Patsogolo Kuuzimu ? Ngati mungabwele kuno , mungapitilize kucita upainiya popanda kukhala na motoka yoyendela . ’ Anthu amene analipo anaona kuti Yesu anali kukonda kwambili Lazalo ndi acibale ake . Pali nkhani zitatu za m’Malemba ouzilidwa zimene mwina anali kuzikumbukila . Iye amadziŵa kuti mtumiki wake wodzozedwa aliyense angakhalebe wokhulupilika ndi kulandila mphoto ya mtengo wapatali imeneyi . Conco , lolani kuti onse a m’banja lanu azibweletsa kwa Yehova nsembe ya “ ana amphongo a ng’ombe ” mlungu uliwonse . 6 , 7 . ( a ) Kodi kuphunzila Baibulo kumalimbitsa bwanji ubwenzi wathu ndi Yehova ? Tiyeni tikambilane mfundo zina zoonjezela zimene zingatithandize kuyankha mafunso aŵili omalizawa . 3 : 14 ) Conco , tisalole kuti cikondi cathu cizilale . Oimila ufumu wa kumwela ndi oimila ufumu wa kumpoto anabwelela nawo limodzi kucoka kuukapolo . ( Ŵelengani Aheberi 5 : 7 , 11 - 14 . ) Abale enanso aŵili amene anali kutumikila m’dipatimenti imeneyi ndi m’bale Robert Wallen ndi Charles Molohan . Conco , Yesuyo adzakuthandizani kuweluza ngati mmene iye amaweluzila . ( Mat . Pa abale anga onse , pali mng’ono wanga mmodzi amene watumikila mokhulupilika monga mkulu kungocokela pamene makonzedwe okhala na akulu pa mpingo anayamba m’ma 1970 . Marita atadandaula kuti Mariya sakum’thandiza , Yesu anamuuza kuti : “ Mariya wasankha cinthu cabwino kwambili , ndipo sadzalandidwa cinthu cimeneci . ” Pa nduna za boma za m’nthawi yake , iyenso amachulidwa pa lemba la Luka caputala 3 vesi 1 . ( Yak . N’cifukwa ciani ena zimawavuta kukhulupilila kuti Yehova amawakonda ? 6 : 7 ) Ndithudi , mtundu watsopano umenewu unali kukulilakulila . Kodi ndi kudziyesa kotani kumene kungatithandize kukhala ndi maganizo oyenela ? Ni utumiki wopatulika uti umene acicepele ambili amasangalala kuucita ? 10 : 16 - 21 ) Ngati munthu amene amadya zizindikilo pa mwambo wa Mgonelo wa Ambuye wacita chimo lalikulu , ayenela kupempha akulu kuti am’thandize mwa kuuzimu . Aaron anayamba kuŵelenga Baibulo mokhazikika , kukonzekela misonkhano na kuyankhapo . Brazil 770,000 Tsiku loyamba pamene tinali mu ulaliki , mayi wina anamvetsela mwachelu . Conco , n’naŵelenga Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . Jane , Danica , Rodney , na Jordan MARCH 3 - 9 , 2014 | TSAMBA 7 • NYIMBO : 106 , 46 ( Aheberi 11 : 32 - 35 ) Kuonjezela pa zitsanzo zakale , tilinso ndi zitsanzo zabwino za abale ndi alongo athu amene ali ndi cikhulupililo . ( b ) Kodi mkwatibwi amamuona bwanji mwamuna wake wamtsogolo ? Zimenezi zimaiŵalika pakakhala mkangano . Ngati timakhala chelu ndi kukwanilitsidwa kwa maulosi a m’Baibo ndiponso zimene Yehova Mulungu ndi Yesu Kristu akucita , sitidzalephela kuona umboni wakuti tikukhala kumapeto kweni - kweni kwa dongosolo lino la zinthu . Potsilizila , adzawonongedwa kothelatu . — Mateyu 25 : 41 ; Chivumbulutso 20 : 1 - 3 , 7 - 10 . Kodi Imfa Ndi Mapeto a Zonse ? Nthawi zambili munthu wokhulupilila ciphunzitso ca Karma amavomeleza mavuto ake ndi a anthu ena popanda kuthedwa nao nzelu . Mwacitsanzo , munthu angalaile kunchito kuti mailo sadzabwela ku nchito , kapena kuti adzakomboka msanga , cifukwa akukaonana ndi dokota . Yomaliza ndi yakuti , kodi zimenezi zikutiphunzitsa ciani ponena za Yehova ndi Yesu ? Ngati munthu amakwiya msanga , akhoza kukhumudwitsa ena . Patapita mawiki angapo , mmodzi wa maticawo anapezeka pa msonkhano wacigawo ku Leipzig . ( Mlaliki 12 : 13 ; Chivumbulutso 4 : 11 ) Tikacita zimenezi , ndiye kuti tacita cinthu camtengo wapatali , ndipo timasangalatsa Mlengi wathu . Mukakonzekela , lembani kalata ku ofesi ya nthambi imene imayang’anila dzikolo kuti akuuzeni zoonjezeleka . Kwa zaka , iye wakhala akusonkhanitsa nkhani za mu Nsanja ya Mlonda , zimene zimakamba za Cikumbutso ndi za cikondi cimene Yehova na Yesu anationetsa . N’zoona kuti sangatithandize mozizwitsa , koma nthawi zonse amatipatsa thandizo limene tikufunikila . Kodi kusakonda Mulungu kwakhala na zotulukapo zotani ? Koma Amai ndi Atate sanandilole kucoka pa nyumba . ( Mateyu 6 : 6 , 8 ) Pa usiku womaliza monga munthu padziko lapansi , Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Ngati mupempha ciliconse kwa Atate m’dzina langa adzakupatsani . ” Ŵelengani Aefeso 6 : 15 . Anadzaza mitima yanu ndi cakudya komanso cimwemwe . ” ( Mac . Koma mnzanga amene ndinali kukhala naye m’cipinda cimodzi anali kundilimbikitsa . ( Aroma 6 : 17 , 18 ) Conco , ifenso tili “ ngati akufa ku ucimo . ” Mwina Eliya anadabwa ataona zimene Ahabu anacita pamene anamva ciweluzo ca Mulungu . Kuphunzitsa ena n’kofunika kwambili cifukwa ciŵelengelo ca anthu amene ayamba kutumikila Yehova cikuwonjezeka . Ngakhale kuti a Mboni ali ndi zofooka ndipo amalakwitsa zinthu zina , Yehova amawatsogolela ndi mzimu woyela . 21 : 5 . Koposa zonse , iwo sanaiŵale zimene anaphunzila . Anali kukumbukila ndi kusinkha - sinkha malonjezo a Mulungu ndi malamulo ake . Mwacitsanzo , nthawi ina atakumana ndi cikhamu ca anthu , anawamvela cifundo cifukwa “ anali onyukanyuka ndi otayika ngati nkhosa zopanda m’busa . ” Tingacite ciani kuti tipewe tembelelo lolembedwa pa mpukutu wouluka ? Conco , Timoteyo anadziŵa kuti akatengela citsanzo ca Paulo , anthu a ku Lusitara kuphatikizapo atate ake adzamutsutsa . Pa Salimo 41 , Davide anakambanso za nthawi pamene anadwala kwambili cakuti anada nkhawa ndi kufooka . ( Ŵelengani Salimo 139 : 14 . ) Inde , kupatula nthawi yomvetsela nkhani yonse na kuona zimene mungayankhepo kudzakuthandizani kusayankha mopupuluma kapena kucita zinthu mosaganiza bwino . Ngati Yosefe sakanawasonyeza kukoma mtima , mwina io sakanamufotokozela vuto lao . 110 : 3 ; Miy . Cikhulupililo canga na ubale wanga ndi Mulungu zimalimbilako nikaona mmene iye amanisamalila . ” Anthu amasiyana - siyana maganizo ponena za ciŵelengelo ca anthu amene anafa ndi mliliwu , koma ena amanena kuti mliliwu unapha anthu pafupi - fupi 50 miliyoni . DOREEN anadabwa kwambili poona kuti mwamuna wake Wesley , wa zaka 54 , anamupeza na cotupa cacikulu ku ubongo . “ Khote - khote Ngwanjila , Palinga Mtima Mpomwepo ” ( Australia ) , Feb . 8 , 9 . ( a ) N’cifukwa ciani atsogoleli Aciyuda anapempha kuti akhwimitse citetezo pa manda a Yesu ? Pofuna kuteteza mwana wosabadwayo , Maria anathaŵa m’cipatalaco . Mumamva bwanji mukaganizila cikondi ca Yehova pa inu ? 13 : 14 , 20 , 21 ) Ganizilani cabe mmene nkhani za ciukililo zimenezi zinam’khudzila Marita . Mukayang’ana zipatso zakupsa , mukhoza kuona kuti sizifanana ndendende . Amene analemba kalata yacitatu ya Yohane anadzicha “ mkulu . ” N’ciani cimathandiza Kim kupitiliza kuonetsa cifundo mosasamala kanthu za mavuto amenewa ? Mwacitsanzo , tizilalikila za Ufumu wa Mulungu ndi kupanga ophunzila . ( Ŵelengani Ezekieli 38 : 23 . ) 15 , 16 . ( a ) Ni nchito iti ya kubwezeletsa na kuyenga imene yakhala ikucitika m’nthawi yathu ? Zimenezi zapangitsa kuti Nyumba za Ufumu zimangidwe ngakhale m’madela amene mipingo ilibe ndalama zokwanila zomangila Nyumba za Ufumu . ( Ŵelengani 1 Yohane 5 : 3 , 4 ) Ndi cinthu ca nzelu kumutumikila mokhulupilika panopa . Coyamba , anayamba kusonkhana mu mpingo wa Cifulenchi . Coyamba , ganizilani citsanzo ca Yakobo . Davide anamvela , ndipo ananyamuka kupita ku Cigwa ca Ela atanyamula cakudya cokapatsa abale ake . Kodi Ufumu umaonetsa bwanji kuti Mulungu amatikonda ? NYIMBO : 88 , 120 N’cifukwa ciani tingakambe kuti Yehova ali ndi cikondi cosatha kwa anthu ake ? Tidzaona cifukwa cake kulimbikitsana n’kofunika maningi masiku ano . Baibulo lili ndi mabuku opatulika okwana 66 . N’nali kukumbukila mau a mtumwi Paulo a pa Aroma 12 : 21 , akuti : ‘ Musalole kuti coipa cikugonjetseni , koma pitilizani kugonjetsa coipa mwa kucita cabwino . ’ Izi zinanikhumudwitsa kwambili . Msonkhano uliwonse umatithandiza kudziŵa zambili ponena za Yehova . 4 : 3 ) M’nyengo ino ya Cikumbutso , komanso maka - maka pa tsiku la Cikumbutso , tiyenela kuganizila mmene timacitila zinthu na ena . Mau amenewa aonetsa kuti Inoki anali kuopa Mulungu ngakhale kuti anali kukhala ndi anthu osaopa Mulungu . Ndiye cifukwa cake Baibulo limatikumbutsa kuti , anthu a Yehova afunika ‘ kupatuka pa zinthu zoipa . ’ Nanga bwanji za kukhala oona mtima ? Kuti mudziŵe zambili za mmene mungakhalile na umoyo wokondweletsa Mulungu , onani nkhani 12 m’buku imeneyi , Zimene Baibulo Ingatiphunzitse yofalitsidwa na Mboni za Yehova . Ezara anaona kuti zinthu zimenezi zinali zopeleka zaufulu zopita kwa Yehova . Conco , anayesetsa kucita zinthu mosamala pofuna kuteteza katunduyo pa ulendo wawo wodutsa m’dela loopsa . Kodi zinthu zinali bwanji pakati pa Ayuda ku Yerusalemu pambuyo pakuti Zekariya waona masomphenya a namba 7 ? Tinadziŵa kuti nthawi zina zidzakhala zovuta kusunga lonjezo limeneli . Nthawi zingapo , atate anadzanditenga ku likulu la apolisi n’kupita nane ku nyumba . Ndinali kukangana kwambili ndi anthu . ( Yakobo 4 : 8 ) M’nkhani ino , tikambilana njila zinai zimene Yehova amationetsela cikondi cake . ( 2 Akor . 3 : 17 ) Davide anakamba kuti : “ Ulemu ndi ulemelelo zili pamaso pake [ pa Mulungu ] , pokhala pake pali mphamvu ndi cimwemwe . ” Buku lina linafotokoza luso linalake limene anthu a mu mzinda wa Galileya anali kugwilitsila nchito kuti asunge bwino nsomba . Yesu anati : “ Odala ndi anthu amene amabweletsa mtendele . ” Ni umboni uti umene uonetsa kuti Mulungu anali kutsogolela Bungwe Lolamulila m’zaka 100 zoyambila mofanana ndi mmene akutsogolela a m’Bungwe Lolamulila masiku ano ? Makolo amene amakonda ana ao ayenela kuwalanga akalakwitsa . Molingana ndi golide , mkuwa kapena kuti kopa , ni mwala wonyezimila wamtengo wapatali . Posapita nthawi , asilikali aciyuda analoŵa mu Yerusalemu , na kupha kagulu ka asilikali aciroma . Kenako iwo analengeza ufulu wawo kwa Aroma . Kodi nzelu za Yehova zimaposa bwanji nzelu za anthu a m’dziko lolamulidwa na Satana ? Zotulukapo zake , uthenga wa Ufumu umene uli ngati mbewu unazika mizu mumtima mwathu na kukula n’kukhala monga mmela wa tiligu . Kwa zaka zambili , magazini ino yafotokoza kuti atumiki a Mulungu amakono analoŵa mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu mu 1918 , na kuti anamasulidwa mu ukapolowo mu 1919 . Iye anaona monga kuti Yehova akumuuza kuti : “ Nimakukonda , osati cabe cifukwa ndiwe mpainiya , komanso cifukwa ndiwe mwana wanga , ndipo unadzipeleka kwa ine . Komabe , zovala zathu ziyenela kukhala zooneka bwino , zoyela , zaulemu , zogwilizana ndi cocitikaco , ndi zovomelezeka kumaloko . Tayesetsa kucita zonse zimene tinali kuona kuti ni cifunilo ca Yehova , ndipo umenewu wakhala umoyo wokhutilitsa . Aŵiliwa anali kukhala mumzinda wa Uri pamodzi ndi acibale awo , ndipo anali na nyumba yawo - yawo . ( Maliko 13 : 15 - 18 ) Kodi ifeyo tidzalolela kusiya kapena kulandidwa zinthu zina kuti tidzakhalebe okhulupilika kwa Mulungu ? “ Anthu ambili ali monga akadoli otsatsila malonda a zovala mu shopu . Uthenga umene uli pa Yesaya 41 , poyamba analembela anthu a Mulungu akale . Pewani zotangwanitsa . Ngakhale kuti Yesu anaponya Satana padziko lapansi , iye akalibe kutsiliza kugonjetsa . ( Chivumbulutso 6 : 2 ; 12 : 9 , 12 . ) Womasulila wabwino afunika kudziŵa zimene wolemba nkhani afuna , ndipo zimenezo ziyenela kukhudza mmene angamasulile nkhaniyo . Baibo imayelekezela mabungwe amenewo na mapili ndi zilumba cifukwa ambili mwa iwo amaoneka olimba ndi osasunthika kwa anthu a m’dzikoli . 19 : 9 ) Onani nkhani yakuti “ Lingaliro la Baibulo : Chigololo — Kukhululukira Kapena Kusakhululukira ? ” A Yohane : Iyai . Yehova amatisamaliladi . Kodi ndimalemekeza makonzedwe a Mulungu a ukwati ? Nthawi zambili , wamasalimo Davide anali kuthandizidwa na mzimu woyela wa Mulungu . 15 : 3 - 8 . Asa ndi Yehosafati Tifunika kukhala naye pa ubale wolimba . Conco , Rabeka anathamangila kunyumba kwa mai ake kukawafotokozela zonse zimene zinacitika . — Genesis 24 : 22 - 28 , 32 . “ Muzicita zimenezi pondikumbukila . ” — 1 AKOR . Malinga ndi zimene munaphunzila m’Baibulo , mumadziŵa mmene tiyenela kuonela munthu wocotsedwa . N’cifukwa ciani Akhiristu afunika kuyesetsa kukhala odziletsa ? Kodi Mboni za Yehova zimapemphetsa ndalama ku Nyumba zao za Ufumu kapena pamisonkhano ikuluikulu ? Yakobo 1 : 5 imati : “ Ngati wina akusoŵa nzelu , azipempha kwa Mulungu , ndipo adzamupatsa , popeza iye amapeleka mowoloŵa manja kwa onse ndiponso amapeleka mosatonza . ” Abulahamu anali ndi cikhulupililo colimba cifukwa anali kuganizila za kukwanilitsidwa kwa ulosi wa Mulungu wokhudza “ mbeu ” yolonjezedwa . ( Gen . Ndipo monga ciwombankhanga cimene cimauluka m’mwamba kwambili , muzidalila Mulungu amene amapeleka ciyembekezo cimene cingakupatseni mphamvu . Iye yekha ndi amene akanatha kuuzila mpweya wa moyo m’zinthu zonse . — Yobu 33 : 4 . “ Vulani umunthu wakale pamodzi ndi nchito zake . ” — AKOL . ( 2 Maf . 15 : 7 , 32 ) Nkhani ya Azariya imapezekanso pa 2 Mbiri 26 : 3 - 5 , 16 - 21 . Kuwonjezela pa kupempha zosoŵa zathu , kodi tifunika kupemphelelanso ndani ? ( Gen . 3 : 15 ) Udani pakati pa njoka ndi mkazi udzakhala waukulu cakuti Satana adzayesetsa kuononga mbeu ya mkazi . Ine n’nali na mnzanga amene anali kunithandiza tsiku lililonse . ( Chiv . 17 : 5 - 7 ) Baibulo limayelekezela zipembedzo zonse zonyenga ndi hule , ndipo izi n’zoyenela cifukwa atsogoleli a machalichi amacita cigololo cauzimu ndi atsogoleli a maiko a m’dziko loipali . Timangofunikila kukhala ndi zotulukapo zake kwa umoyo wathu wonse . 11 : 20 ) Ponena za Cikumbutso cimeneci , ena angafunse kuti : N’cifukwa ciani timakumbukila imfa ya Yesu ? Yehova amene anayambitsa cikwati , wapeleka malangizo abwino kwambili kwa amuna ndi akazi kudzela m’Baibulo . — Ŵelengani 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 . Mofananamo , ngati ifenso timayesetsa kuona zimene abale amacita bwino , naonso adzalimbikitsidwa ndipo adzacita zambili mu utumiki wao kwa Yehova . Vikwati vina vakhala pamavuto , kapena kutha ndithu , cifukwa mmodzi wa aŵiliwo amakonda kutamba zamalisece . Musalole kuti munthu akuposeni mphamvu . ” Nanga tiyenela kucita ciani kuti tizikhulupilila kuti njila za Yehova n’zolungama ? Yona anati : “ Pamene ndinalefuka kwambili , ndinakumbukila Yehova . ” — Yona 1 : 3 , 10 ; 2 : 1 - 9 . N’zoona kuti nthawi zina panali kucitika nkhondo monga mmene Yesu anakambila . Kodi Yesu anasankha kucita ciani ? Nanga anakwanilitsa bwanji zimenezo ? Ndipo tingayambe kutengeka pang’ono - pang’ono n’kucoka kwa Yehova . Kodi iwo anamvetsa cifukwa cake sanafunike kuphwanya fupa lililonse ? ( 2 Tim . 3 : 1 - 5 ) Makolo ena sayamikila ana awo cifukwa makolo awo sanali kuwalimbikitsa . Iye anati : “ Pamene tinawatumila foni kuwauza zimene zinacitika , ambili a io anabwela patangopita cabe mphindi 45 . Kucita zimenezi kumawathandiza kukonzekelelatu mphatso yabwino koposa imene angakapeleke pa cocitika ciliconse . ( January 1 , 2014 ) . Tinali kuzinyamulila mu saka yonyamulilamo mbatatisi , yochedwa mishok . Panthawi ina , Yehosafati anacita zinthu mopanda nzelu mwa kugwilizana ndi Mfumu Ahabu ya Isiraeli pankhondo yofuna kulandanso mzinda wa Ramoti - giliyadi m’manja mwa Asiriya . Anthu amaona kuti dayamondi ni mwala wa mtengo wapatali . Kenako , a David anasiya kupezeka pamisonkhano . Zimenezi zinandikondweletsa kwambili . N’cifukwa ciani misece ni yoopsa ? DANIEL NA MIRIAM anakwatilana mu September 2000 , ndipo anali kukhala mu mzinda wa Barcelona , m’dziko la Spain . Bwanji ngati ana anu sapita patsogolo ? Nanga bwanji ngati amakaikila ubale wao ndi Yehova ? Kodi mungacitenji ? “ Tamandani Yehova , inu angelo ake amphamvu , ocita zimene wanena , mwa kumvela malamulo ake . ” — Salimo 103 : 20 . Mandy ananidziŵikitsa kwa Horst na Angelika , amene anali a Mboni . Banjali linanithandiza kumvetsetsa Mau a Mulungu . N’kutheka kuti ena anafika pomazilambila . ( Gen . Zimenezi zingakuthandizeni kupewa kudziona kuti ndinu wosafunika kwa Mulungu . Iye anachula mfundo zofunika m’malo mongokamba mwacisawawa . Patsiku lina Antoine anatsala pang’ono kufa atatsekeledwa ndi cimwala . Munthuyo anali Yesu . Timatengako mbali pa kuthandiza ena . M’buku la Masalimo , Mulungu akunenedwa kuti ni “ wacifundo ndi wacisomo . ” Iye “ sadzakhalila kutiimba mlandu nthawi zonse cifukwa ca zolakwa zathu , kapena kutisungila mkwiyo mpaka kalekale . ” Anthu okhawo amene anali kudzakhala Anaziri , monga Samisoni , ndiwo amene sanali kugela tsitsi lawo . — Numeri 6 : 5 ; Oweruza 13 : 5 . Ganizilani citsanzo ca mlongo Irene wa ku United States , amene sali pabanja . 6 : 9 , 10 ) Cifukwa cokonda Mulungu , anatula pansi udindo wake ndi kuleka khalidwe logonana ndi akazi anzake . Ndi makhalidwe ati amene muona kuti ndi ofunika kwambili kuti anthu asangalale mu cikwati ? Pamisonkhano , timaphunzila Baibulo ndipo Yehova amatiuza zimene tiyenela kucita , ndi mmene tiyenela kukhalila paumoyo . Tikhoza kupilila mayeselo amenewa malinga ngati tidalila Mulungu . ( 1 Pet . Ngati ana anu akukumana ndi ziyeso monga kuuzidwa kuimba nao nyimbo yafuko kapena kucita zikondwelelo za dziko , muyenela kuwathandiza mwamsanga . 8 MUNTHU AMENE MUKONDA AKADWALA MATENDA OSACILITSIKA ( Machitidwe 10 : 34 , 35 ) Mulungu amaona anthu onse cimodzi - modzi . Izi zathandiza kuti maganizo anga akhale ogwilizana kwambili na maganizo a Yehova . ” Akawauza kuti acite cinthu cina cake , anali kuwafotokozela cifukwa cake ayenela kucita zimenezo . Pamene atumwi anali m’ndende , mngelo anatsegula zitseko za ndendeyo , na kuwauza kuti apitilize kulalikila m’kacisi . — Machitidwe 5 : 17 - 21 . Anali kupemphela kwa Yehova mocondelela kuti awapatse mphamvu zowathandiza kupilila . ( Aef . 6 : 4 ; Sal . 127 : 3 ) Mosiyana ndi ana a mu Isiraeli wakale , ana a Mboni akabadwa sakhala mbali ya anthu odzipeleka a Yehova . Tifunika kukonda kwambili Baibulo cifukwa ndiye njila yaikulu imene Mulungu amalankhulila nafe . Mwina anthu ena anadabwa kuona kuti dziko la Iguputo , mmene anthu anali kucita zamatsenga ndi kukhulupilila mizimu , linakhala ufumu wamphamvu padziko lonse koma anthu a Yehova anali akapolo m’dzikolo . N’ciani cina cimene mungasinkhesinkhe ? 14 , 15 . ( a ) Kodi Paulo anatilimbikitsa kuika maganizo athu pa ciani ? ’ Tsopano ndinali ndi mwai wodziŵa kusiyana pakati pa zimene alongo ao a atate anali kukhulupilila ndi za m’machalichi ena . Mtumwi Petulo anati : “ Nonsenu muzicitilana zinthu modzicepetsa , cifukwa Mulungu amatsutsa odzikweza , koma odzicepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu . ” — 1 Pet . Iwo anayamba kukondana kwambili moti palibe cimene cikanasokoneza ubwenzi wao . A Zulu : Cabwino , onani zimene vesi lotsatila likunena . Ngakhale kuti sindikumasulilanso , ndimayamikila Yehova pondilola kupitilizabe kucilikiza nchito yomasulila mabuku padziko lonse . Cikondi cidzatilimbikitsa kuika zofuna za ena patsogolo , ngakhale kuti kucita zimenezi kungafune kuti tidzimane zinthu zina zimene mwalamulo n’zololeka kwa ise . — 1 Akor . Anthu a m’madela amenewo anali kulambila milungu yambili . — Agal . N’cifukwa ciani tiyenela kuyamikila akulu mumpingo ? Mulimonse mmene zingakhalile muyenela kufufuza cithandizo ca okalamba kwanuko . Zotsatilapo zake n’zakuti anthu amene amamumvela adzakhala ndi cimwemwe ceniceni . Yehova ndiye woyenela kulamulila cilengedwe conse cifukwa ni Mulungu wamphamvuyonse ndiponso ni Mlengi . Pa kuphunzila kwanga Baibulo zaka zonsezi , nthawi zonse ndimayesa kuti ndione ngati ndikali kukhulupilila mfundo zimenezi . Sanafunike kutenga zinthu zikulu - zikulu zimene abulu na ngamila zingalephele kunyamula , komanso wosafunikila pa umoyo wosamuka - samuka . * Koma , kodi Rabeka anadziŵa kuti ngamilazo zinali ndi ludzu kwambili ? Ndiponso timam’konda ndi mtima wathu wonse , maganizo athu onse , ndi mphamvu zathu zonse Mosamala , mboni ingayambe makambilano ndi munthu wina mwa kukambako za nyuzi , kuyamikila khalidwe la ana ake , kapena kum’funsako za nchito yake . ( Aroma 3 : 2 ) Mulungu anauzila amuna okhulupilika kulemba mabuku amenewa pa nthawi yaitali . Anawalemba pafupi - fupi zaka 1,100 kuyambila mu 1513 B.C.E . mpaka ca kumapeto kwa caka ca 443 B.C.E . Nanga zimenezo zinathetsa bwanji mantha ake ? Yesu anakamba fanizo la mfumu imene inakhululukila kapolo amene anakongola ndalama zambili zokwana madinari 60 miliyoni . Ndipo mphatso imeneyi inatsegula mwai wakuti anthu azitha kukhala pa ubwenzi ndi Yehova . Ni mfundo yanji imene Paulo anaphunzitsa abale a ku Filipi m’kalata imene anawalembela ? Nanga ise tiphunzilapo ciani ? Mwacitsanzo , mayi akhoza kumathela nthawi yaitali akusamalila mwana wake . A Inoki : M’mau ena ndinganene kuti mfundo za m’Baibulo n’zothandiza masiku ano monga mmene zinalili zaka zambilimbili zapitazo pamene linalembedwa . Baibulo linalembedwa ndi anthu 40 . Zimene io analemba zili ndi mfundo yaikulu imodzi ndipo sizitsutsana . Pokhala opanda ungwilo , tonse timalakwa . Baibulo limati : “ Kuti anthu adziŵe kuti inu , amene dzina lanu ndinu Yehova , Inu nokha ndinu Wam’mwambamwamba , wolamulila dziko lonse lapansi . ” Ndi madalitso otani amene tiyembekezela mtsogolo ? Anacitadi momwemo . ” — Eks . MOUZILIDWA , mtumwi Paulo analemba makhalidwe 9 amene mzimu woyela umabala . ( Agal . ( Luka 22 : 42 ) Tiyeni titengele citsanzo ca Yesu coseŵenzetsa ufulu wathu kulemekeza Yehova ndi kucita cifunilo cake . Kodi kuŵelenga ndi kusinkhasinkha nkhani ya Hezekiya kungatipindulitse bwanji ? 2 : 21 ) Mulungu sangasangalale ngati ife tipeleka ulemu wopambanitsa kwa anthu . Ngati nthawi zonse makolo sakhala ndi nthawi yolankhula ndi ana ao , ana m’banja angalephele kuwauza mavuto ao . Ena ali pa maudindo , zingawavute kugaŵilako acinyamata maudindo . Atate ŵake a Yesu ni Mulungu , amene dzina lake ni Yehova , ndipo “ nyumba ” yake ili kumwamba . Wamasalimo anati : “ Cilungamo ndi ciweluzo ndizo maziko a mpando [ wake ] wacifumu . ” Conco , tili na cikhulupililo cakuti malamulo ake , mfundo zake , ndi zigamulo zake , zonse n’zolungama . Ngati zinthu zingakhale conco , ndiye kuti anthu amene sakhulupilila Baibulo angavomeleze kuti ulosi wa m’Baibulo ukukwanitsidwa . Mulungu analosela kuti Koresi anali kudzagonjetsa mitundu ya anthu , kudzamasula Ayuda mu ukapolo , ndi kuwacilikiza panchito yomanganso kacisi woyela . Ngakhale kuti anali mfumu yochuka monga mtengo umene unakula mpaka kufika kumwamba , iye anadulidwa mpaka patadutsa “ nthawi zokwanila 7 . ” Kulankhula za Yehova ndiponso kum’tamanda poyela ndi mbali zofunika kwambili pa kulambila kwathu . — Aheb . N’zosangalatsa kwambili kudziŵa kuti Akristu oona oposa 8 miliyoni akutamanda Yehova mwacangu masiku ano . Ndi masinthidwe ena ati amene anapangidwa mu Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso ? ( Aroma 8 : 37 - 39 ) N’zoona kuti nthawi zina timalema . Monga mmene malamulo a zacilengedwe sasinthila , Yehova nayenso sasintha . Mau a Mulungu amatithandizanso kudziŵa kuti mapeto ali pafupi . Cifukwa ca kupanda cilungamo kumeneku , anthu ena acilitidwa nkhanza zosaneneka . M’kupita kwa nthawi , ana anu adzayamikila kwambili zimene mumawaphunzitsa . * ( Mat . 24 : 14 ) Fanizo la Yesu la wofesa mbewu limatsimikizila mfundo imeneyi . Ataphunzila Baibo , Patricia amene tam’gwila mau kuciyambi anaphunzila kukhululukila ena . Rute anapeleka citsanzo cabwino pa nkhani imeneyi . ( Aheb . 12 : 14 ) Zimenezi zimaphatikizapo kukhala pa mtendele ndi abale athu . Yesu anati : “ Conco , ngati wabweletsa mphatso yako paguwa lansembe , ndipo uli pomwepo wakumbukila kuti m’bale wako ali nawe cifukwa , siya mphatso yako patsogolo pa guwa lansembe pomwepo . ▪ Kupyolela m’Baibulo , mwacikondi Mulungu amatiuza zimene tingacite kuti atiyanje ndi zimene tingacite kuti ‘ tidzathe kuthawa zinthu zonse zimene zikuyembekezeka kucitika . ’ — Luka 21 : 36 ; Yohane 17 : 3 . [ Cithunzi papeji 4 ] Cipupa comangidwanso pa mabwinji a Nineve wakale [ Eni ake ] Randy Olson / National Geographic Creative [ Cithunzi papeji 5 ] Zimene aneneli analosela za kugwa kwa Babulo zinacitika ndendende Zosankha zina zimene tingapange zingatipangitse kukhala akapolo a nkhongole kwa zaka zambili . Komabe , cifukwa cofunitsitsa kuyambanso utumiki wanthawi zonse , iwo anagulitsa bizinesiyo , boti , ndi katundu wina . Apa m’pamene n’natengela coonadi kukhala canga - canga . ” Kenako , anayesa kumukhazika mtima pansi dilaivayo , koma sizinathandize . Mwacionekele , simukanacita zimenezo . Kodi aliyense payekha afunika kuyesetsa kucita ciani ? Tonse tiyenela kucita zimene tingathe kuti mpingo ukhalebe wogwilizana . 14 , 15 . ( a ) Kodi Petulo anacita ciani atayamba kumila ? Tsikulo , kunali kotentha kwambili , koma banja lokalamba limeneli mwamsanga linapita kukalandila alendo . Pamafunika khama kuti tipeze mau abwino amene tingakambe . Iye anazindikila kuti ngakhale kuti anali kudzimva monga munthu wophwanyika , akanatha kuthandiza ena . Yehova anauzila Lamekiyo kukamba ulosi wokhudza mwana wake Nowa , ndipo ulosi umenewo unakwanilitsika pambuyo pa cigumula . ( 2 Akor . 4 : 7 ) Ndipo cacinai , Atate wathu wacikondi wakupatsani ubale wapadziko lonse wa alambili oona amene ‘ amapitilizabe kukutonthozani ndi kukulimbikitsani . ’ Baibulo lamasulidwa m’zinenelo zoposa 2,800 ngakhale kuti anthu ena amafuna kuliononga kothelatu . Monga mmene Baibo inakambila , anthu “ ocokela m’zilankhulo zonse za anthu a mitundu ” akubwela m’gulu la Yehova . ( Zek . 3 : 1 , 2 , 16 ) Zocita zanu zidzathandiza abululu anu kuona kuti a Mboni za Yehova amakhala na vikwati vabwino , amasamalila bwino ana awo , amakhala aukhondo ndi akhalidwe labwino , ndiponso amakhala na umoyo wacimwemwe . Nanga kodi Paulo anatanthauzanji pokamba za “ kuika maganizo pa zinthu za thupi ” ? NYIMBO : 143 , 124 Ngati mwaona kuti muyenela kuongolela kuti muzikhululukila ena , pemphani Yehova kuti akuthandizeni kucita zimenezo . Pocita utumiki wopatulika kwa Mulungu , tiyenela kukhala oyela m’maganizo , m’mitima , ndi matupi athu . Yesu Khiristu anakamba kuti Atate wake wakumwamba amakoka anthu kupitila mwa Mwana Wake . Anthu ambili amaganiza kuti nchito yaikulu ya mwamuna ndi kupezela ndalama banja lake basi . Iwo anali kudela nkhawa zinthu zimene sanafunike kuda nazo nkhawa . Nthawi zina abale ndi alongo ambili amalefuka , amada nkhawa , kapena amadziona kuti ndi acabecabe . Ataona Yosefe , sanamudziŵe , koma iye anawadziŵa . Ulosi wa Yeremiya umati : “ Pa tsiku limenelo padzakhala anthu ophedwa ndi Yehova kucokela kumalekezelo a dziko lapansi kufikanso kumalekezelo ena a dziko lapansi . ” Cifukwa cotsatila malangizo a m’Baibo , lomba tili na umoyo wacimwemwe . ” Mwacitsanzo , analonjeza Abulahamu kuti mbadwa zake zidzakhala m’Dziko Lolonjezedwa . A Hava nawonso anakankhila mlandu kwa njoka , kuti ni imene inamunyenga . ( Gen . Kodi Mboni zinzake zinacita ciani ? Bungwe la padziko lonse limeneli linakhazikitsidwa mu 1908 ku Britain , ndi mkulu wa gulu la nkhondo la ku Britain dzina lake Robert Stephenson Smyth Baden - Powell . Pambuyo pofotokoza zocitikazo , Baibulo limacenjeza kuti : “ Amene akuyesa kuti ali cilili asamale kuti asagwe . ” ( 1 Akor . 11 : 13 - 18 ) Kuwonjezela apo , angelo anali kuthandiza ndi kupititsa patsogolo nchito yolalikila imene bungwe lolamulila linali kuyang’anila . ( Mac . Iye anakhala moyo ndendende monga mmene Adamu anafunika kukhalila — munthu wangwilo , wokhulupilika kothelatu ndi womvela Mulungu . ( 1 Tim . ( Genesis 29 : 10 ) Nthawi zambili , anthu amene amaphunzila kukwela pa ngamila amadandaula cifukwa ca mavuto amene amakumana nao , ngakhale paulendo waufupi . Baibulo limatiuza kuti tizipewa “ nchito za thupi . ” Ambili Adzapulumuka ​ — Nanga Inuyo ? 8 Panthawi ngati imeneyi , tikhoza kumalakalaka kukhala na munthu amene amaoneka kuti amasamala za ise . Kodi zimene ndaphunzila ndingazigwilitsile nchito bwanji . . . Nthawi zambili , lemba la Aheberi 4 : 12 limalembedwa m’zofalitsa zathu pofuna kuonetsa kuti Baibulo ili na mphamvu yosintha anthu . Mpake kuti lembali limagwilitsidwa nchito motele . ( Num . 16 : 23 - 27 ) Ndiyeno , Yehova anapha apandu onse . Nthawi zina mzela wobadwila wa Yesu unali kupitila mwa mwana woyamba kubadwa , koma osati nthawi zonse . mmene timagwilila nchito yolalikila ? Lamulo lalikulu kwambili kwa ise Akhristu ni lakuti tiyenela kukondana . Cifukwa cakuti cimwemwe ceni - ceni ni mbali ya cipatso ca mzimu woyela wa Mulungu . Zimene Asa anacita zionetsa kuti iye anali paubale wolimba ndi wodalilika ndi Yehova . 13 : 12 ) Ngati timaganizila kwambili pa zinthu zimene tinali kuyembekezela koma sizinacitike , tingafooke kwambili . Kodi tingapindule bwanji ndi zitsanzo za anthu okhulupilika a m’Baibulo ? Sitikayikila kuti panthawi imeneyo aliyense , pa dziko lapansi adzaona “ cuma copambana ca kukoma mtima kwake kwakukulu . ” Baibulo limatiuzanso zitsanzo za anthu amene mapemphelo ao anayankhidwa . 1 : 19 , 20 ) Dipo limapatsa anthu onse okhulupilika ciyembekezo ca moyo wamuyaya . 4 : 13 - 15 ) Koma kodi kupita patsogolo nthawi zonse kumatanthauza kulandila udindo wina ? ( Eks . 3 : 11 ) Zaka 40 zimenezi zisanacitike , Mose anali atathaŵa kucoka ku Iguputo ndipo anakhala umoyo wothaŵathaŵa . Ni mmene cikhulupililo cathu cilili . Liu la Cingelezi limene limamasulidwa kuti “ Mdyelekezi , ” linacokela ku liu la Cigiriki limene limatanthauza kuti “ woneneza . ” Kumbukilani kuti Satana safuna kuti inu muziganiza bwino . Pa mwambo wa Pasika , Yesu anauza Yudasi kuti : “ Zimene wakonza kucita , zicite mwamsanga . ” N’cifukwa ciani munasankha kukatumikila ku dziko lina kumene ni kosoŵa ? 3 Kodi Mungathandize Ena Mumpingo Wanu ? N’cifukwa ciani tiyenela kukonda adani athu ? Kodi kukhwima mwakuuzimu kumatanthauza ciani ? Cidzakhaladi cokondweletsa ngako kukhalapo panthawi imene tonse tidzavala bwino - bwino umunthu watsopano tili angwilo ! Ndipo linali kugwilitsidwa nchito bwanji ? Komabe , kambili zikondwelelo zimenezi zimaloŵetsamo zocitika zotsutsana na zimene Baibo imaphunzitsa . ULENDO winanso , mzimayiyo anakalipilanso Toñi . Mwacitsanzo , ngati mumalimbikila kugwila nchito za pakhomo , mumapeputsilako ena zocita m’banja lanu . Kodi ana a Yosiya ndiponso mdzukulu wake anadzakhala anthu otani ? Iwo anali kufuna - funa paliponse , ngakhale m’zakudya zang’ombe . Gulu la Mulungu limapelekanso maphunzilo kudzela m’Sukulu ya Gileadi . Zomelazo zili m’gulu lochedwa Posidonia oceanica , mtundu wa maudzu a m’nyanja amene anamela kwambili pansi pa nyanja ya Mediterranean , pakati pa dziko la Spain ndi Cyprus . Masiku ano , Akristu naonso amapindula ndi malamulo ena . Paul anapitiliza kuti : “ Yesu anati : ‘ Musamade nkhawa za tsiku lotsatila , cifukwa tsiku lotsatila lidzakhala ndi zodetsa nkhawa zakenso . Makalata a mtumwi Paulo amakamba zambili pa nkhani ya ufulu . Ngakhale n’conco , tidziŵa kuti Yehova Mulungu wathu anathandiza atumiki ake akale m’njila imene sanali kuyembekezela , ndipo iye sanasinthe . Abale ndi alongo ambili akhala akutumiza makalata oyamikila kaamba ka Baibuloli ku likulu la Mboni za Yehova ku Brooklyn , New York . Ena ndi amishonale ndipo amathela nthawi yao yoculuka mu ulaliki . ( Luka 12 : 42 ) Amatipatsa cakudya cimeneci kupitila m’zofalitsa zosiyanasiyana zokhala na malangizo othandiza kapena cilango . 3 FUNSO : Kodi mzimu woyela n’ciani ? Mwacionekele , ambili amene anali kuŵelenga Malemba Oyela m’citundu cimene anali kumvetsetsa , anapeza mavesi ena amene anawakonda kwambili . Kuti Yehova akwanilitse zimenezi , anapanga mapangano ena kuti cifunilo cake cikwanilitsidwe . Anthu amene anamugula anapita naye ku Iguputo . Ngakhale kuti io amapeza ndalama zocepa , Yehova amawasamalila nthawi zonse . Pa jw.org mungaŵelenge kapena kucita daunilodi Baibo na mabuku ena osiyana - siyana mahala . Zinthu zimene zinacitika masiku 40 pambuyo pa kuukitsidwa kwa Yesu , zinapeleka umboni wotsimikizilika . M’nkhanizi , tidzaphunzila mmene atumiki a Mulungu angakulitsile ubwenzi wao ndi Yehova n’colinga cakuti akhale Akristu ofikapo . Yehova ndiye amasankha nthawi yodzoza anthu . 5 : 6 , 7 . 12 : 31 ; 1 Yoh . 5 : 19 ) Motelo , zinthu zimene dzikoli limalimbikitsa sizigwilizana ndi mfundo za m’Baibulo . Apo n’kuti patapita wiki imodzi cabe kucokela pamene mumzindawo anaikamo maloboti . Conco , tonse timafunika kulimbikitsiwa nthawi na nthawi . Tikhale Ogwilizana Pamene Mapeto a Dzikoli Ayandikila , 12 / 15 Tsanzilani Cikhulupililo ca Mose , 4 / 1 Kodi tingaphatikizepo zinthu ziti podzifunsa kuti , ‘ Kodi ine nimakonda ciani maka - maka mu umoyo wanga ? ’ Aisiraeli anakhala bwanji ‘ mtengo wa mpesa wacilendo ’ kwa Yehova ? Kodi galamafoni inali kugwilitsidwa nchito bwanji ? Yehova anakondwela ngako na zimene munacita patsikulo . Kodi Akristu amene atumikila kwa zaka zambili ayenela kudzifunsa funso liti ? Mafunso amenewa adzayankhiwa m’nkhani yotsatila . Koma ngati mkazi apeza nthawi yabwino yofotokozela mwamuna wake zinthu zosakondweletsa mwaulemu , mwamunayo adzamuyamikila na kum’konda kwambili . Poli anati : “ Ndinataikilidwa mwamuna wanga wokhulupilika amene ndinakhala naye m’cikwati zaka 33 . ” ( b ) Kodi pamene tigwila nchito yolalikila , timakhala okonzeka kucita ciani ? Yesu atamaliza kudya Pasika womaliza pamodzi ndi atumwi ake , iye anacita pangano ndi ophunzila ake okhulupilika . * — Ŵelengani Afilipi 2 : 19 - 22 . Ngakhale zinali conco , n’napitiliza kuphunzila Baibulo ndipo sin’nalole wina aliyense kapena cina ciliconse kunibweza m’mbuyo . Atatulutsidwa anabwelela ku Karítsa . Kumeneko mkulu wanga , Ilias , anamufunsa mafunso ambili okhudza Baibo . Imati : “ Kuleza mtima kumanyengelela mtsogoleli wa asilikali , ndipo lilime lofatsa likhoza kuthyola fupa . ” — Miy . 3 : 12 ) Koma ngati ticiikako nzelu , cikhulupililo cathu cidzapitiliza “ kukula , ” cakuti tidzakhala “ acikhulupililo colimba . ” — 2 Ates . Kuti afalitse coonadi ca m’Baibo m’zinenelo zosiyana - siyana , mu 1884 kunakhazikitsidwa bungwe la Zion’s Watch Tower Tract Society . Enanso akuvutika cifukwa cosiyana cipembedzo ndi anthu a m’banja lao kapena cifukwa cokhala m’banja la kholo limodzi . Iye akumbukila zocitika zosiyanasiyana pamene makasitomala ndi ocita zamalonda anali kucita zinthu mwacinyengo pokambilana ndi akuluakulu a boma . Zimenezi n’zofunika kuti akwanilitse nchito yao yaikulu . Kwa zaka zambili , Yehova wakhala ndi gulu limene limam’tumikila mokhulupilika . Kodi nimalabadila mofulumila malangizo ocokela kwa otiyang’anila ndi kuwacilikiza ? ’ — w16.11 , peji 11 . Kugwila nchito yomanga kungakuphunzitseni mmene mungapewele ngozi , kukhala wakhama pa nchito , na kugwilizana ndi okutsogolelani . Mwa njila imeneyi , ndiye kuti mudziphunzitsa kucita zinthu zoposa pa zimene muyembekezeleka kucita , osati kucita kukukakamizani koma mwa kufuna kwanu . — Mateyu 5 : 41 . ▪ Muzisinkhasinkha za Cikondi Cosatha ca Yehova Wolemba Salimo 71 : 9 anacondelela Mulungu kuti : “ Musanditaye nthawi ya ukalamba wanga . Ame . ” — Chiv . Cifukwa caciŵili cimene timakhulupilila kuti Yesu anaukitsidwa n’cakuti tili ndi umboni wa anthu ambili . ( Aroma 7 : 24 , 25 ; 8 : 2 ) Mofanana ndi Paulo , na ise tiyenela kuyamikila kwambili kuti Yehova anatimasula ku ukapolo wa ucimo na imfa . Ndiyeno , Mdyelekezi ndi onse amene adzam’tsatila adzaonongedwa kwamuyaya pa “ imfa yaciŵili . ” Tidzapewa ciliconse cimene cingaticititse kukhala ndi cikhumbo cofuna kugonana ndi munthu amene si mwamuna kapena mkazi wathu . Koma n’nafunikabe kucoka . M’bale angapemphe wacicepele amene adziŵa bwino kugwilitsila nchito kompyuta kuti apulinte nkhani pa webusaiti ya jw.org zimene zingalimbikitse acikulile amene alibe kompyuta . Cifukwa ca ici , cinali covuta kwa ena kuvomeleza njila yatsopano yolambilila kapena kuleka zinthu zosayenela zimene anali kucita . Koma anapewa kutengela zilakolako na zolinga za anthu amene anali kukhala nawo . Ofalitsa pafupifupi 1,100 amatumikila m’mipingo 35 ndi m’tumagulu 15 ndipo amagwilitsila nchito cinenelo ca Cingabere . Iwo analibe ciyembekezo ciliconse . Conco n’nali kulakalaka kuwauza za Ufumu wa Mulungu . Zinthu zonse zimene ndikupanga n’zatsopano . ” Popeza kuti Ayuda ambili anayamba kukamba Cigiriki , cinakhala covuta kwambili kuti azimvetsetsa Malemba Aciheberi . N’zacisoni kuti , m’kupita kwanthawi Aisiraeli anasiya kumvela malamulo a Mulungu . N’ciani cimene atumiki a Yehova amakonda kucita ? Kuti timvetsetse mfundo za m’nkhani imene tidzaphunzila , tifunika kukonzekela bwino phunzilo lililonse la Nsanja ya Mlonda . M’maiko oculuka , anthu ambili amene akubatizidwa ndi acinyamata . Yehova amayamikila kudzipeleka ndi kukhulupilika kwathu kwa iye . Sitiyenela kutalikilana ndi Yehova . Kodi Mulungu Angayankhe Mapemphelo Anga ? Paulo anali wofunitsitsa kudziŵa zimene “ anthu oculuka ” anali kuganiza mu ulaliki . Tifunika kukumbukila kuti pamene Satana anaponyedwa pansi kucokela kumwamba , iye anadziŵa kuti watsala ndi kanthawi kocepa . Kamnyamata ka m’nthano imeneyo kanaonetsa khalidwe limene likanapindulitsa akulu - akulu . Ndipo zimenezi zimaononga banja . 4 : 7 - 9 ) Kodi zitsanzo za m’Baibo zimene takambilana zitiphunzitsa ciani ? Izi n’zogwilizana n’zimene Yohane analemba . “ Onetsani kuwala kwanu pamaso pa anthu , kuti . . . alemekeze Atate wanu wakumwamba . ” — MAT . Tingadziŵe bwanji kuti sitikunyala - nyaza nchito ya Yehova ? Zina mwa nkhani zimene zafalitsidwa ndi izi : “ Kodi Mzimu Woyela N’ciani ? ” Aya ni mafunso ofunika kwambili amene tiyenela kuwaganizila m’nyengo ino ya Cikumbutso . TATE amaphunzitsa bwino ana ake ngati iye ndi citsanzo cabwino . Mzimayiyu analoŵa m’cigulu ca anthu mwakacete - cete , n’kufika kumbuyo kwa Yesu , na kugwila kunsi kwa covala cake . Dzina la mtumiki ameneyu ndi Eliezere . Nanga kuganizila zocitika zimenezo komanso ciyembekezo cimene anthu ena okhulupilika akale anali naco , kuyenela kukhudza bwanji ciyembekezo canu ? Mneneli Yesaya analosela kuti mu ulamulilo wa Ufumu , anthu ‘ sadzavulazana kapena kuwonongana , ’ kapenanso kuononga dziko lapansi . Kodi kukhala ndi cithunzi m’maganizo mwathu ca mphoto yosaoneka kungatithandize bwanji masiku ano ? Nanga masiku ano anthu a Yehova aphunzilapo ciani pa uphungu wouzilidwa wa Paulo ? MUZIONA THUPI LANU NA MOYO WANU KUKHALA MPHATSO YAMTENGO WAPATALI . Robert , Luis , Raquel , ndi Julian anapeza citonthozo , ngakhale kuti anakumana ndi mavuto aakulu . Iye sanamvetsetse cifukwa cake asilikali a Mulungu wamoyo , Yehova , anali kuthawa munthu wamba wopembedza mafano . Zina zimene analemba n’zakuti : “ Lelo nadziŵa dzina la Mulungu . Tidzakambilana zocita za akazi ena oopa Mulungu a m’nthawi yakale . 37 : 18 - 28 ) Kodi mukuona ciani ? Mukumvela zotani ? M’baleyu anapilila mavuto aakulu m’ndende zozunzilako anthu za Nazi . Iye analemba kuti : “ Ndinaona mngelo winanso akuuluka capafupi m’mlengalenga . Iye anali ndi uthenga wabwino wosatha woti aulengeze monga nkhani yosangalatsa kwa anthu okhala padziko lapansi , ndi kudziko lililonse , fuko lililonse , cinenelo ciliconse , ndi mtundu uliwonse . ” Malangizo ao anandithandiza kwambili cakuti sindimaononga ndalama zambili . ” Mmene Danieli anadziŵila Yehova . 34 : 18 ) Kulankhula mwa njila imeneyi kungalimbikitse aja amene akufunikila citonthozo . — Miy . Michael ndi Olga ali ndi Marina ndi Matthew Zimenezi zimatithandiza kuti tizilalikila mosavuta uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . ( 2 Akorinto 4 : 4 ; 1 Yohane 5 : 19 ; ŵelengani Chivumbulutso 12 : 9 , 12 . ) Ku Isiraeli , anthu akamva dzina lakuti Sisera anali kucita mantha kwambili . Popeza lomba tadziŵa kuti kupanga lonjezo kwa Mulungu ni nkhani yaikulu , tiyeni tikambilane mafunso aya : Ndi malonjezo ati amene ise Akhristu tingapange ? Goliyati , anayamba kupita kumene kunali Davide . Cifukwa ca khalidwe lathu labwino , tinadalitsidwa kuona anthu amene anatigwila akulemekeza dzina la Yehova . — 1 Pet . NYIMBO : 148 , 109 Mwacitsanzo , kodi tingadziŵe bwanji kuti ndise okhwima mwauzimu ? N’cifukwa ciani tinganene kuti Kristu anakwela pahachi ‘ cifukwa ca kudzicepetsa ’ ? Sitikukaikila ngankhale pang’ono kuti mwa thandizo la Mulungu tingapilile ziyeso kapena mavuto amene tingakumane nao tsopano kapena mtsogolo . N’namvetsa kuti Mulungu amatipatsanso nyumba yauzimu , malo a citetezo ceni - ceni kumene tingapeze mabwenzi eni - eni okonda Yehova , amene angatilimbikitse . Ndinayamba kuda nkhawa kwambili . Ulendo wina apolisiwo atabwela , anali kucoka ciŵe , cifukwa tsikulo kunapsa kwambili , ndipo zovala zawo zinafipa ngako . Anacititsa kuti anthu mumpingo ayambe kukangana pa mau ndipo mumpingo munaloŵa mzimu woipa . Iye anacita zimenezi mwa kupeputsa lamulo limene anthu anafunikila kumvela . Pa cifukwa cimeneci , amuna ambili amaona monga kuti akunyalanyazidwa na mkazi wawo , popeza kuti mkaziyo amatangwanika ndi kusalamalila mwana . Kodi “ anamwali anzake ” a mkwatibwi amagwila nchito bwanji limodzi ndi otsalila a Akristu odzozedwa ? Motsogoleledwa ndi mzimu woyela wa Mulungu , io anafika ku Torowa . Ana ake akuluakulu anapita kukadyetsela ziŵeto kufupi ndi Sekemu kumene anakumana ndi adani pasanapite nthawi . Mungatumize copeleka canu kudzela ku banki kapena pogwilitsila nchito makadi a kubanki . Ndipo ndimafunika kucotsamo zina tsiku lililonse . Ndikafufuza zimene zili m’maganizo mwanga , nthawi zambili ndimapezamo ‘ maganizo olefula . ’ Iwo adzakuthandizani kuganizila maluso amene muli nao ndiponso zolinga zanu . Nkhondo imene tikumenya ni yauzimu osati yakuthupi . “ Pa mlingo umene munacitila zimenezo mmodzi wa abale anga aang’ono awa , munacitila ine amene . ” — MAT . ( Mat . 24 : 14 ) Tsopano tiyeni tikambilane zinthu zimene zidzacotsedwa Ufumu wa Mulungu ukadzabwela . ( Yobu 2 : 4 , 5 ) Cifukwa ca zimene Mdyelekezi anakamba , Yehova walola kuti anthu adzilamulile n’colinga cakuti adzionele okha kuti kudzilamulila kumabweletsa mavuto aakulu . Mukakumana ndi mayeselo , kodi mumayamikila cisamalilo cacikondi cimene Yehova amapeleka ndi kum’dalila kuti iye adzakuthandizani kupilila ? — 2 Akor . Iye anali kufunitsitsa kuti Ayuda ena akapulumuke . Pakatulutsidwa cofalitsa catsopano , anali kuulutsa pa mawailesi a boma , ndipo nthawi zina cofalitsaco cinali kukhala mutu wa nkhani pa nyuzi . Kwa zaka 15 , iye anali kuba . Koma analeka . Kuonjezela apo , “ mnofu ndi magazi sizingaloŵe ufumu wa Mulungu . ” Ndiye cifukwa cake Yesu anayelekezela kukhala wotsatila wake ndi kunyamula goli . Pamene munayesedwa kuti mucite zinthu zoipa , kodi munakwanitsa kusiyanitsa coyenela ndi cosayenela ? Dziŵani kuti Yehova amakondwela nanu . ( 1 Pet . 3 : 1 - 4 ) Conco , ngakhale pamene zinthu si zili bwino , mungatamande Yehova ndi kupita patsogolo kuuzimu . Zotelo zikacitika , pitilizani kuyembekezela Yehova kuti akulimbitseni . Kodi Paulo anaonetsa bwanji kuti anali wofunitsitsa kupilila ? Iye amafunika kukhala ku oksijini kwa maola 16 pa tsiku . Yesu amamvela Mulungu ndi kucita cifunilo Cake . M’pemphelo lake la citsanzo , cinthu coyamba cimene Yesu anachula ni kuyeletsedwa kwa dzina la Mulungu . Koma maganizo amenewo anali ngati kunyoza Yehova . Iye amaona mitima ndipo anaona kuti m‘mitima mwao munali cinyengo . — Yer . [ Bokosi papeji 7 ] Zimene Mulungu Walosela Raymond , amene tam’chula poyamba , anati : “ Ngati munthu amafunitsitsa kukhala wochuka zimavuta kuti akhale wokhutila . Mwacitsanzo , timaphikila , kuotha , ndi kuunikila . M’malomwake , ndimamuthandiza kuti acite bwino nchito yake youza anthu mau a Mulungu . ( Sal . 51 : 17 ; 94 : 18 , 19 ) Yehova ndi Yesu amamvelela cisoni anthu onse ovutika . Anthu amene anakhala Akristu ku Lusitara , ayenela kuti anakondwela kwambili atadziŵa za ciyembekezo cimene otsatila a Kristu anali naco . Malipoti a m’maiko ambili aonetsa kuti kusakhala pamodzi monga banja kwabweletsa mavuto aakulu . Yesu Kristu anakamba mau amenewa kwa bwanamkubwa waciroma wa Yudeya pamene anali kumzenga mlandu . Amene anali kutumikila m’bungwelo anali atumwi poyamba . Ndipo tikulimbikitsa ena kuti naonso aciteko utumiki umenewu . ” Ndipo ngati aphunzitsiwo anali kufuna kuyesa Yesu mwa kum’funsa mafunso odzutsa mikangano , io analephela . N’ciani cinathandiza anthu monga Daniel ndi Andre kukhala ndi maganizo oyenela pa nchito ? Dziko lapansi lili ndi njila yapadela yothandiza anthu , zinyama , ndi zomela kukhala ndi moyo . Popeza kuti zofalitsa zathu timazigaŵila mahala , ena amaona kuti kukopela zofalitsazi na kuziika pa mawebusaiti ena kapena pa malo ocezela a pa intaneti kulibe vuto . Tonse tili na ucimo wobadwa nawo , koma timafuna kucita zinthu zokondweletsa Yehova . ▪ ‘ Mvelani ndi Kumvetsa Tanthauzo Lake ’ Baibo imatilimbikitsa . . . Ngakhale kuti mwamuna ndiye mutu wa mkazi , Baibulo limakamba kuti iye ayenela kulemekeza mkazi wake . Kuona zinthu moyenelela n’kofunika ngako kuti tipitilize kuika maganizo athu pa nkhani yaikulu , ndi kucilikiza ulamulilo wa Yehova . Mfundo yakuti sanafunike kuda nkhawa , koma anafunika kupemphela kuti alandile mtendele wa Mulungu . Akanani ambili anali kulambila Baala , mulungu wonama amene iwo anali kukhulupilila kuti ndiye anapanga moyo ndi kuti ndiye mulungu wa makumbi , mvula , ndi mphepo . 16 : 22 , 23 ) N’cifukwa ciani Yesu anachula Petulo kuti “ Satana ” ? ( 1 Sam . 15 : 22 ; Miy . ( 1 Samueli 2 : 12 ) Eli anali kudziŵa kuti ana ake akucita zinthu zoipa kwambili . 1 / 1 “ Uzikonda Mnzako Mmene Umadzikondela Wekha , ” 6 / 1 ( Ŵelengani Yohane 11 : 32 - 35 . ) Baibo imakamba kuti m’manda amenewo anali asanaikemo munthu cikhalile . Pamene tinali kuphunzitsa anthu Malemba , ambili analabadila . Fanizo la Yesu la mtumiki wosalungama n’locititsa cidwi . Izi zingatipangitse kuganiza kuti pamene Rehobowamu anamvela uphungu wa Mulungu , mwina anacita zimenezo cabe cifukwa cosonkhezeledwa ndi anthu ena , osati cifukwa colapa na mtima wonse kapena kufuna kukondweletsa Mulungu . ( Ŵelengani Miyambo 2 : 1 - 5 . ) Yehova amatilonjeza kuti adzapeleka “ njila yopulumukila ” ngati sitinyalanyaza mfundo za m’Baibulo ngakhale pamene tili pa mavuto . Pophunzitsa ana anu muyenela kucitapo kanthu mwamsanga mukaona mbali zimene sacita bwino . 10 : 12 , 13 . M’bale Mumba : Mungafunse . Anali kulalikila Ayuda cifukwa anali kuwadela nkhawa kwambili . Baibulo limakamba kuti Yehova ndi Yesu amaonetsa cifundo ndi cikondi cacikulu . Matendawa amachedwa kuti cerebral palsy ( CP ) . Dzinali amaligwilitsila nchito kuchula matenda okhudza ubongo amene amalepheletsa munthu kuyenda ndi kucita zinthu zina . Ifotokoza cifukwa cake kupezeka pamisonkhano kumatipindulitsa , kumathandiza ena , ndi kukondweletsa Yehova . N’ciani cinathandiza Asa kudalila kwambili citsogozo ndi citetezo ca Mulungu ? Mkambi anapeleka citsanzo ca mpingo wa mumzinda wa St . Koma “ anamumvela cisoni , ” ndipo anaganiza zomulela monga mwana wake . — Eks . Ayuda ambili pa nthawiyo anali na maganizo amenewo . * Zimenezi zingoonetsa kuti anthu analengedwa kuti azikonda zinthu za kuuzimu . Kodi mumathela nthawi yaitali bwanji pocita zosangulutsa ? Ngati moto wophikila cakudya uyenela kuyang’anilidwa bwino kuti usabweletse ngozi , kodi n’ndani amayang’anila kutentha kwa dzuŵa ? ’ Pa mfundo zimene takambilana , mwina tikumva mmene atumwi anamvelela pamene anapempha Yesu kuti : “ Tionjezeleni cikhulupililo . ” Mwacitsanzo , ganizilani za dzuŵa limene analenga . 3 : 16 ) M’caputala ciliconse ca buku limeneli , dzina la Yehova limachulidwa pafupifupi nthawi 10 . Kuti mmene ucimo unalamulila monga mfumu pamodzi ndi imfa , momwemonso kukoma mtima kwakukulu kulamulile monga mfumu kudzela m’cilungamo . N’cifukwa ciani ndife ocimwa ndipo timafa ? Tifunika kumakamba zinthu zoyamikila Yehova . Mungacite ciani ngati mumayesedwa kuti mucite ciwelewele ? Conco anacita zosakhulupilika kwa Yehova Mulungu wake ndipo anapita m’kacisi wa Yehova kukafukiza paguwa lansembe zofukiza . ” Kodi lonjezo la Yehova la pa 1 Akorinto 10 : 13 limakulimbikitsani bwanji ? Iwo anali kumbuyo kwanga , ndipo sin’namve ngakhale kuti anakuwa . Makolo anga anali ndi ana 8 . Ine n’nali mwana wawo wa namba 7 . Ngakhale kuti anali ofunitsitsa kulalikila , sanali kudziŵa zimene angakambe . Vuto limeneli linayamba kalekale . Kodi tingaonetse cikhulupililo m’njila ziti ? ( b ) Tiphunzilapo ciani pa citsanzo ca Julien ? Ndinali kuganiza kuti palibe amene anali kudela nkhawa zimene zinali kucitika ku Vietnam . “ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” Mpainiya wapadela ali m’mbali mwa nyanja ku Las Terrenas , ndipo akuseŵenzetsa Baibulo kulalikila munthu amene wacoka kukolola ma kokonati Tifunika kuyamikila kuti Yesu anapeleka moyo wake monga dipo limene limatipatsa mwai wodzakhala ndi moyo wosatha m’dziko latsopano la Mulungu . 17 - 19 . A Zulu : Mwakamba zoona , ndi mmenedi zilili ! Mpingo wina wa ku Canada unalemba kuti : “ Nkhani yakuti ndife ‘ mboni za Yehova ’ yatikondweletsa kwambili , ndipo yaticititsa kukhala ofunitsitsa kucita zinthu mogwilizana ndi dzina lathu latsopano . ” Iye amatipatsa malamulo cifukwa amatikonda . Koma azibusawo sanagwilizane nazo . ( 1 Akorinto 14 : 23 - 25 ) Yehova amatsogolela misonkhano yathu ndi mzimu wake woyela , ndipo zimene timaphunzila zimacokela kwa iye . Ufumu umenewu udzaononga adani a Ufumuwo amene ndi maboma andale . Yosimbidwa ndi Felisa ndi araceli fernández Mulungu walola kuti maboma a anthu akhalepo cifukwa cakuti amathandiza kuti m’dziko mukhaleko bata ndi mtendele . Ndiyeno muonetseni phunzilo logwilizana ndi nkhaniyo m’kabuku ka Uthenga Wabwino . Ndinali kuganiza kuti ndingapeze mayankho a mafunso anga m’mabuku oculuka a Cijelemani amene amafotokoza zinthu mozama . Olo kuti Aroni ndiye anapanga fanolo , iye analapa na kukhala ku mbali ya Yehova pamodzi na alevi anzake . Ngati makolo ao ndi Mboni , mwacionekele amafunitsitsa kuti ana ao apitilize ndi utumiki wao wanthawi zonse . Tiyeni tipitilize kukhala na cikhulupililo m’malonjezo a Yehova . ( Onani pikica pamwambapa . ) ( b ) Kodi Mwanawankhosa wochulidwa pa Chivumbulutso 5 : 13 n’ndani ? Palibe cina cofunika kwambili kuposa kukhala mtumiki wa Mulungu . Zimene Akristuwo anacita , zitiphunzitsa kufunika kophunzila Baibulo ndi zofalitsa zathu mosamala . 15 : 3 ) Tiyeni tionenso njila zina zoonetsela kuti ndife okhulupilika kwa Mulungu . Mtumwi Yohane anaona masomphenya a “ angelo anai ataimilila m’makona anai a dziko lapansi . Kodi mfundo zimenezi ndingazigwilitsile nchito bwanji paumoyo wanga ? Ciyembekezo cimathandizanso kwambili kuti munthu athetse maganizo odzipatula na kudziona kuti palibe amene angamuthandize , komanso kuthetsa mantha , ” inakamba conco buku yakuti , Hope in the Age of Anxiety . * . . . m’masautso athu onse . ” — 2 AKOR . 1 : 3 , 4 . ( Mlaliki 9 : 11 ) Kwa zaka zambili , nkhondo , ciwawa ndi matenda zapitiliza kupha anthu abwino . Monga mmene tidziŵila , Kaini sanapange cosankha cabwino . Iye anakamba kuti mbali zonse za thupi ndi zogwilizana “ mwa mfundo iliyonse yogwila nchito yake yofunikila . ” ( Yakobo 1 : ​ 19 ) Iwo ayenela kuzindikila mmene ana ao akumvela , ndipo angazindikile zimenezi ngakhale kudzela m’zimene anao angalankhule . ​ — Ŵelengani Numeri 11 : ​ 11 , 15 . Mwa kukonda Mulungu ndi anzathu , timalemekeza zimene Yesu anakamba pankhani zofunika zimenezi . N’cifukwa ninji ? ( b ) Kodi “ mau a Mulungu ndi amoyo ” motani ? Tingasinthenso zinthu zina paumoyo wathu kotelo kuti tizilalikila ku magawo amene samalalikilidwa kaŵilikaŵili . Munthu amene anatiitana angakhale kuti wakonzekela kale zambili , ndipo tingamuonongetse zinthu zambili ngati tasintha maganizo . Dale anati : “ Khalani ndi umoyo wosalila zambili , ndipo mudzasangalala paumoyo wanu wonse . ” ( Aef . 6 : 11 ) Ndiye cifukwa cake tiyenela kutsatila cenjezo la pa 1 Petulo 5 : 9 limene limati : “ Khalani olimba m’cikhulupililo ndipo mulimbane naye . ” Zimatikhudza cifukwa cakuti zimatipatsa ciyembekezo ca zinthu zabwino zamtsogolo . Ngakhale n’conco , timawalemekeza abale amenewa cifukwa cakuti amatumikila mwakhama ndipo ni odzicepetsa . — Ŵelengani 2 Akorinto 1 : 24 ; Chivumbulutso 19 : 10 . Onani Nsanja ya Olonda yacingelezi ya June 1 , 1987 , masamba 30 - 31 . Kapena kodi anali kufuna kutiphunzitsa zinthu zinazake zimene zingakhale zothandiza m’masiku otsiliza ano ? Iye anapezamo mabuku ofotokoza Baibulo . ( Num . 12 : 3 ) Zimene zinacitika zinaonetsa kuti Farao anali munthu woipa mtima ndi wodzikuza . ( Eks . Mungakumane ndi mavuto aakulu kwambili , n’kuyamba kuona kuti simungathe kupilila . Ndipo kuti mphatso ioneke kuti ni yamtengo wapatali zimadalila woilandila . Nthenda yoopsa imeneyi inali kuwononga minyewa ya munthu wodwalayo n’kumupundula . Iwo anati : “ Zimenezi zacokela kwa Yehova . ” Kuwonjezela apo , olo kuti anthu ena amakamba momasuka zimene amakonda na zimene sakonda , nthawi zina sangakambe zosoŵa zawo . 19 : 11 - 21 ) Kodi zimenezi zikusonyeza kuti cikwati cidzacitika Mfumu isanamalize nkhondo yolimbana ndi adani ake ? ( Miyambo 2 : 21 , 22 ) “ Taonani ! Komabe , anthu aciguami , amene nyumba zawo zinali m’mbali mwa njila anali kuwalandila bwino , maka - maka pamene anadziŵako mau ena m’citundu cawo . Nafenso tingapindule kwambili ngati tikhulupilila kuti dipo ndi mphatso yathu yocokela kwa Yehova . Ndi zocitika zapadela ziti zimene zinali kucitika pamene bukuli linali kulembedwa ? CIKONDI cozikidwa pa mfundo za m’Baibo ( a·gaʹpe ) ni mphatso yocokela kwa Yehova . Masomphenya amenewa adzakuthandizani kudziŵa amene ‘ amakhala ’ kumwamba . Tonse tadziŵa kuti ni nthawi yokhala pansi ndi kumvela nyimbo zamalimba pulogalamu ikalibe kuyamba . Kodi pangano la mu Edeni limatitsimikizila ciani ponena za njoka ndi mbeu yake ? A Inoki : Cinali cifukwa cakuti kupatulapo Baibulo panalibe maumboni ena otsimikizila kuti iye anali munthu weniweni . Munthu wakupha mnzake mwangozi anali kufunika kukhalabe mumzinda wothaŵilako mpaka mkulu wa ansembe akamwalile . — Num . 137 : 1 , 3 ) Izi ziyenela kuti zinali kuwapweteka mumtima Ayuda okhulupilika monga Danieli . Ana sapindula ndipo amakhumudwa ngati mumasinthasintha powalanga . Mwa ici , angalephele kupeleka ulemelelo kwa Mulungu . — Aroma 15 : 1 - 3 ; 1 Tim . Ngati mwamuna na mkazi amagwilizana amakhala monga woyendetsa ndeke na wom’thandiza wake amene onse ali na colinga copita ku malo amodzi . Ambili mwa mabuku amenewa anawalemba m’Ciheberi , ndiye cifukwa cake cigawo cimeneci timacicha Malemba a Ciheberi , cimadziŵikanso kuti Cipangano Cakale . KUKOMA MTIMA Tili na mwayi wouza anthu onse za madalitso okondweletsa amene ali pa Chivumbulutso 21 : 4 , 5 akuti : “ [ Mulungu ] adzapukuta misozi yonse m’maso mwawo , ndipo imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . Tsiku na tsiku anali kuyanjana ndi atsikana ambili ocokela kumadela onse a ufumu wa Peresiya . ( b ) Kodi mwapindula motani cifukwa comvetsela ana anu ? Kenako , iye anayamba kundifotokozela zimene Baibulo limakamba zakuti akufa adzauka . N’nali kukonda kuvala manja a pulastiki kuti nizioneka kuti nili na manja . Conco kuyambila mu 1943 , mipingo inayamba kucita Sukulu ya Ulaliki . Komabe , ngati palibe mfundo za m’Baibulo zimene zanyalanyazidwa , anthu a Yehova amapewa kukangana ndi ena pankhani zimenezi . M’malo moika maganizo ake pa “ zinthu zapadziko , ” Abulahamu “ anakhulupilila mwa Yehova . ” Komanso , ena salandila uthenga wathu poopa kunyozedwa ndi anthu a m’dela lawo kapena abululu awo . 18 Woweluza wa Dziko Lonse ” Amacita Cilungamo Nthawi Zonse TSAMBA 19 Mwanjila imeneyi , tinadziŵana ndi Mboni zina zoyambilila za mtundu wacikigizi . Ndise oyamikila kwambili kuti Yehova watipatsa cuma cauzimu . Cuma cimeneci ciphatikizapo , ( 1 ) Ufumu wa Mulungu , ( 2 ) utumiki wathu wopulumutsa moyo , ndi ( 3 ) coonadi camtengo wapatali copezeka m’Mau ake . Colinga ca wopeleka mphatso . ( Ŵelengani Mlaliki 4 : 12 . ) Kuganizila funso lomalizali n’kothandiza kwambili cifukwa cakuti munthu amasangalala kwambili ndi nchito yake ngati akuona kuti ikupindulitsa anthu ena . Kodi panthawi ina ndinapepesa kwa anzanga cifukwa cowatumila zinthu zolakwika kapena zabodza ? Panthawi imene anamasulidwa m’ndende ku Roma ca m’ma 61 C.E . , Paulo anali atagwila nchito yake ya umishonale mwakhama ndi kupilila mayeselo ambili . Malingalilo okhudza kugwila nchitoyi anapelekedwa m’buku lakuti Millennial Dawn Volume 6 ( 1904 ) ndi m’magazini ya Zion’s Watch Tower ya August 1906 , ya m’Cijelemani . 4 : 10 ( Onani ndime 17 - 19 ) Mulungu anaonetsanso cikondi cake cacikulu kwa mtundu wonse wa anthu pamene analamula Nowa kukhala “ mlaliki wa cilungamo . ” ( 2 Pet . Kodi Yesu anapeleka citsanzo cotani pankhani yosamalila amai ake ? Ndinazindikila kuti ndinalibe ufulu wocita zinthu pandekha , moti ndimangokhalila kudziimba mlandu . ” Sitifuna kucita zinthu zimene zingakhumudwitse abale athu kapena kufooketsa cikhulupililo cao . Pamene ticita zimenezi , tiyeni tipeze mayankho pa mafunso awa : Kodi cikhulupililo cinathandiza bwanji Mose kukaniza zilakolako zathupi ? Tikapeza yankho la funsoli , kudzakhala kosavuta kudziŵa pamene Ufumu wa Mulungu unayamba kulamulila . Zocitika zimene Mateyu analemba zokhudza kubadwa kwa Yesu ndi umoyo wake ali mwana zimasiyanako ndi zimene Luka analemba . Cifukwa cake n’cakuti polemba , iwo anasumika maganizo awo pa zocitika zokhudza anthu aŵili osiyana . N’cifukwa ciani Akhiristu ayenela kuganizila mmene mavalidwe awo angakhudzile olambila anzawo ? Kodi pamakhala zotulukapo zanji ngati tionetsa kuwala kwathu ? Kodi Akristu angagonjetse bwanji ciyeso cakuti apite ku dziko lina kukafunafuna ndalama zambili ? 1 : 5 - 8 ; 4 : 8 . “ Ndikatopa pambuyo pogwila nchito , ndimasangalala ndipo ndimaona kuti ndacita zinthu zofunika . Anthu onse adzayankha mlandu pamaso pa Yehova cifukwa ca zocita zawo , maka - maka anthu odziŵika na dzina lake . Kodi abale amene akuphunzitsidwa angatengele bwanji citsanzo ca Elisa ? 7 : 21 , 22 . Anna anati : “ Cinanisonkhezela ni nkhani yokhudza dziko la Myanmar ya mu Buku Lapachaka la 2013 . ” 2 : 21 - 23 , 26 . Nkhani izi , zidzafotokoza mmene tingapewele mzimu wodzikonda wa m’dzikoli mwa kupitilizabe kukonda Yehova , Baibo , ndi abale athu . Vesi imeneyi siikamba kuti mukuyenda pamodzi ndi Yehova ndipo iye wakugwilani dzanja , ngakhale kuti zimenezo zingakhale zosangalatsa . Zimene Mulungu Wakucitilani “ Pakuti Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha , kuti aliyense wokhulupilila iye asaonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” — Yohane . 3 : 16 . Alisa “ Iye ndi Thanthwe , ndipo nchito yake ndi yangwilo , njila zake zonse ndi zolungama . ” — DEUT . Mwamuna wina wa zaka za m’ma 60 anauza wofalitsa wina kuti : “ Ndaŵelenga bukuli nthawi zambili ndipo landitonthoza . Kukhala wodzicepetsa n’kofunika kuti munthu akwanitse kukhululukila ena . Roger , amene anakukila ku malo amene ali pa msenga wopitilila makilomita 1,600 kucokela kwawo , anakamba kuti : “ Cinthu cofunika cimene mungacite kuti mujaile mu mpingo watsopano ni kupita mu ulaliki kaŵili - kaŵili . Monga mmene Yehova anathandizila Hezekiya , Yosefe , ndi Sara , ifenso angatithandize kupilila mavuto amene angaoneke monga osapililika malinga ngati tikhalabe okhulupilika kwa iye . Masiku ano , Akristu anzathu sangaticilitse mozizwitsa . 5 : 22 , 23 . Mwacikondi Sara anakamba zimene zinali zofunikila . Paulo anawauza kuti “ mtendele wa Mulungu . . . umaposa kuganiza mozama kulikonse . ” Anasangalala kuona mmene Yehova anali kuvumbulila coonadi ca m’Baibulo kwa anthu odzicepetsa ngakhale kuti anali osaphunzila . Mwacitsanzo , mu 1932 , Bennett Brickell wa zaka 23 , anacoka ku tauni ya Rockhampton mumzinda wa Queensland ndi kupita kumpoto kwa mzindawo kukalalikila kwa miyezi isanu . ( b ) Tingaonetse bwanji kuti ndife oleza mtima ? Zimenezi zimatisangalatsa kwambili . ” Kenako iye sanaonekenso , cifukwa Mulungu anam’tenga . ” Kodi iwo anali kuona kuti kucita zimenezi kunali kuwalanda ufulu ? Pambuyo popanga ubwenzi ndi anthu amenewa , takhala ndi mwai wokambilana nao kaŵilikaŵili . ” 1 : 29 ) Baibo imakamba kuti Yesu ni wapamwamba kwambili kuposa mafumu onse kapena anthu onse amene anakhalapo mafumu . Komanso iyenela kukhala yomasulidwa molongosoka . Nthawi zambili , aja amene anatsitsidwapo monga akulu , amakhala abusa abwino kwambili kuposa kale . KUMVETSETSA MULUNGU Ponena za mmene munthu wakhungu amadziŵila dziko , mai wina analemba kuti : “ Munthu wakhungu amaphunzila zinthu m’njila zosiyanasiyana monga ( kugwila , kununkhiza , kumva ndi zina zotelo ) , ndiyeno amafunika kuika pamodzi zinthu zimene adziŵa kuti apange cimodzi . ” Iwo anakondwela kwambili ataona kuti Paulo wadzuka , ndi kuti walimba mtima kupitanso mumzinda umenewo . Iwo amaimila zolengedwa zamphamvu zakumwamba zimene zinawononga mzinda wa Yerusalemu ndipo zidzawononganso dziko loipa la Satanali pa Aramagedo . Ngati timakhululukila ena , timalimbitsa mgwilizano ( Onani palagilafu 12 , 13 ) Kodi zocitika zimaonetsa ciani ? Izi zinacititsa anzanga ena m’kilasi kukhumudwa n’kuyamba kuninena . Ndinaona kuti ndifunika kucoka m’gulu la zigaŵenga . N’zoona kuti kuphunzila citundu cina kumatenga nthawi , ndiponso kumafuna khama ndi kudzicepetsa . Cikhulupililo tingaciyelekezele ndi moto . Iye anapemphela kuti : “ Inu Mulungu wanga , limbitsani manja anga . ” Onani Salimo 72 : 16 ; 1 Timoteyo 6 : 8 ; Aheberi 13 : 5 , 6 . Yesu anali ndi mphamvu youza ophunzila ake zocita . N’zoona kuti Akristu ena anakwatiwa kwa anthu amene satumikila Yehova , omwe ndi okoma mtima komanso ololela . 2 : 6 , 7 ) Koma kodi tingacite bwanji zimenezi ? Palibe angatsutse kuti imfa sinafalikile kwa “ anthu onse , ” monga mmene Baibo imakambila . ( 1 Yoh . 2 : 15 , 16 ) Komanso , umacititsa anthu ofooka mwauzimu kunyalanyaza zizindikilo zoonetsa kuti tsiku lalikulu la Mulungu lili pafupi . M’malomwake , tidzafunika kugwilizana kwambili ndi abale athu . ( Mac . 16 : 1 - 3 ) Patapita miyezi yocepa kucokela pamene Timoteyo anakhala mmishonale , Paulo anam’pempha kuti apite ku mpingo watsopano ku Tesalonika kumene abale anali kuzunzidwa mwankhanza . 3 : 13 , 14 . 55 : 2 . Amadziŵanso mtundu wa zakudya zimene thupi limafunikila . Mlongo Lucy atamva zimenezo , anakhumudwa kwambili cakuti anapempha nzelu kwa abale ofikapo . Mkulu wina amenenso ndi mpainiya dzina lake Victor anati : “ Pamene ndinali wacinyamata mkulu wina anandifunsa mafunso ocepa ndiponso osankhidwa bwino okhudza zolinga zanga . Tikalandila alendo , nthawi zambili tinali kucita maseŵela a nkhani za m’Baibo , ndipo pamene ana athu anali kukula , anali kukonda kwambili nkhani za m’Baibo . Timoteyo anakonda coonadi cifukwa cakuti anaganizila zimene anaphunzila ndipo anakhutila nazo “ Valani zida zonse zankhondo zocokela kwa Mulungu kuti musasunthike polimbana ndi zocita zacinyengo za Mdyelekezi . ” — AEF . Yesu anakamba kuti ngati tidzimana zinthu zina cifukwa colambila Yehova , tidzadalitsidwa maningi . — Maliko 10 : 28 - 30 . 11 : 40 ) Komanso , ciŵelengelo cawo cikulila - kulila . Kodi Nowa anaonetsa bwanji kuti anali kukhulupilila kuti Yehova adzamuthandiza kupeza zosowa za banja lake ? ( Ŵelengani Yakobo 1 : 13 - 15 . ) 27 Cikondi — Khalidwe Lamtengo Wapatali Koma mzimu ndi coonadi si zooneka ndi maso , ndipo sizikhala pamalo ena ake . Yesu Khristu anakamba kuti , “ uthenga wabwino uyenela ulalikidwe coyamba . ” Nimakwanitsa kucita zonse zofunikila tsiku lililonse , koma zimatenga nthawi yaitali , ndipo zimafuna khama ndi mphamvu zambili kuposa mmene munthu ali na manja amacitila . Yehova amacitapo kanthu mwamsanga kuti ateteze anthu ake cifukwa ndi a mtengo wapatali kwa iye Adani a Mulungu amacititsa anthu kuti asadziŵe dzina lake . — Yeremiya 23 : 27 . Cinaniŵaŵa ngako cakuti n’nayamba kudziona monga munthu wolephela pa zinthu zauzimu . Ganizilani zimene Yesu anakamba popemphela kwa Atate wake pa lemba la Yohane 17 : 26 . 1 , 2 . ( a ) Kodi Yesu anakamba ciani za masiku otsiliza ? mu Nsanja ya Olonda ya October 1 , 2009 . [ Bokosi papeji 12 ] Iwo angaganize kuti taleka kuwakonda poona kuti siticita nawo zikondwelelo za pa maholide . Ndiponso ngati mufuna kuthandiza abale anu amene si Mboni kuti adziŵe Yehova , mufunika kucita zinthu moleza mtima . Sitima inanyamuka 02 : 00 usiku , ndipo tinayenda maola 6 tisanafike potsikila . Titatsika , tinayenda mtunda wa makilomita 10 kuti tikafike pamalo osonkhanila . ” Mar . “ Kodi izi zindiphunzitsa ciani ponena za Yehova ? ” Yesu anapeleka yankho yomveka bwino pamene anauza omutsutsa kuti : “ Atate wanu Abulahamu anali wosangalala poyembekezela kuona tsiku langa , ndipo analiona moti anakondwela . ” ( Yoh . Ngakhale n’conco , anali kukayikila kuti Yehova amam’konda . Cofunikanso kwambili ni kuuzako ena zimene mwaphunzila . Anthu a ku Yudeya komanso a ku Galileya anali kuona Asamariya monga anthu apansi , ndipo anali kuwasala . — Yoh . Cioneka kuti Sila nayenso anali nzika ya Roma . — Mac . 16 : 37 . Nkhani ya mmene coonadi cinafikila m’dziko la Kyrgyzstan na kufalikila ndi yocititsa cidwi kwambili . M’bale Pryce Hughes amene anamamatila kwa Mulungu ndi kupitilizabe kuyendela limodzi ndi gulu lake anakamba kuti : “ Ndikuthokoza kwambili kuti ndacita mogwilizana ndi cidziŵitso ca zifuno za Yehova kuyambila m’masiku oyambililawo 1914 asanafike pamene zonse zinali zosadziŵika bwino kwambili . . . kufikila lelo pamene coonadi cikuwala ngati dzuŵa lamasana . Iye anakhulupilila kuti mphamvu ya Mulungu idzam’thandiza monga mmene inacitila kwa Yesu . Mulungu anauza mwamuna wokwiya ameneyu kuti ngati angasinthe ndi kucita cabwino , iye adzamuyanja . Zimene mungacite ngati anthu ena akukuvutitsani Afarisi anali kungoganizila colakwa cimene munthu wacita osati mtima wake . ( Mlal . 3 : 12 , 13 ) Popeza tinakokedwa na Yehova , timadziŵa colinga cimene ali naco pa ise . ( Akol . ( Yesaya 48 : 17 , 18 ) Conco , timatsatila kwambili mfundo zimenezo . KUONONGA NCHITO ZA MDYELEKEZI ( b ) N’ciani cionetsa kuti Mulungu akuthandiza gulu lake kupita patsogolo ? Ngakhale n’conco , anavomeleza kuti anali wocimwa . N’ciani cimene Mboni za Yehova zacita kuti zimasulile Baibulo ? Ndipo nthawi zina ndinali kugwilako nchito mu hotelo imeneyi kuti ndizigwilitsila nchito zimene ndinali kuphunzila m’kalasi . Zimenezi zinandidabwitsa kwambili popeza kuti inu mumakamba kuti zonse zimene mumakhulupilila ndi za m’Baibulo . Cimatilimbikitsa kucita zabwino ndi kutithandiza kupewa zoipa . 7 : 39 . Mukasankha kuyenda na Mulungu mmene Inoki anacitila , na kulola Mau ouzilidwa a Mulungu kukutsogolelani pa umoyo wanu , mudzasiyila banja lanu citsanzo cabwino cofunika kutengela . 3 - 5 . Amene anapangitsa zimenezi ni womasulila Baibo wina dzina lake Jacques Lefèvre d’Étaples ( m’Cilatini , Jacobus Faber Stapulensis ) . M’kupita kwa nthawi , iye analembela mnzake kuti : “ N’zocititsa cidwi kuona mmene Mulungu wathandizila [ anthu ] wamba m’madela osiyana - siyana kulandila Mau ake . ” Iye anati : “ Ambili anali aakulu msinkhu kuposa ine , ndipo anandithandiza kwambili . Ilaria akukumbukila kuti pamene anali wacinyamata , anali kufuna kuceza kwambili ndi anzake a kusukulu , koma anadziŵa kuti kucita zimenezo n’kulakwa . Ndinali kulengeza uthenga wabwino wa Ufumu mwacangu pena paliponse . Tiyenela kukhulupilila Yesu ndi kumumvela kuti ‘ tikakhale ndi moyo wosatha . ’ Akhristu amayesetsa kupeza njila zodzitetezela , koma pocita zimenezi , amatsatila mfundo za m’Baibo . Maseŵela a Baseball * anali mbali ya umoyo wanga . Kutonthoza Olila 6 Iwo anapatsidwa ulamulilo pa gawo limodzi la magawo anayi a dziko lapansi , kuti aphe anthu ndi lupanga lalitali , njala , mlili wakupha , ndi zilombo za padziko lapansi . ” — Chivumbulutso 6 : 8 . Kodi Mulungu anam’dalitsa bwanji Yesu “ kosatha ” ? Tsiku lililonse , Yefita ndi mwana wake ayenela kuti anali kukumbukila mavuto amene Aisiraeli anakumana nao cifukwa cosamvela Yehova . Iye ni atate wanga , bwenzi langa , wonitonthoza , ndi mphamvu yanga . N’naona kuti Baibulo ingathandize banja lathu , conco n’nayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . ( Onani palagilafu 12 - 14 ) Mau anu amandikondweletsa ndi kusangalatsa mtima wanga , pakuti ine ndimachedwa ndi dzina lanu , inu Yehova Mulungu wa makamu . ” Motelo , zioneka kuti Paulo ndi Akristu ena anali kuwadziŵa anthu ambili amene anamva mwacindunji pamene Yesu anali kulamula ophunzila ake kuti azilalikila . 27 : 1 - 3 ; 1 Maf . 7 : 13 - 16 ) Conco , m’pomveka kuti mapili aŵili ophiphilitsa amenewa ni amkuwa . Zimenezi zitikumbutsa kuti ulamulilo wa Yehova wa cilengedwe conse komanso Ufumu wa Mesiya ni maulamulilo abwino kwambili , amene adzabweletsa mtendele na madalitso kwa anthu onse . Muzibweza mwamsanga nkhongole iliyonse imene muli nayo Koma Yehova sanafune kumana anthu ake mkate . Atawapatsa cakudya ca m’maŵa , Yesu anafunsa Simoni Petulo kuti : “ Simoni mwana wa Yohane , kodi umandikonda ine kuposa izi ? ” Anthu ena amakhulupilila kuti chimo limene Adamu anacita linali cigololo . Atandipempha kukasonkhana ku Nyumba ya Ufumu ya Mboni za Yehova ndinavomela . Kumvetsa tanthauzo la fanizo limeneli kungatithandize kuti tisakhumudwe kapena kulefuka ngati munthu amene tikuphunzila naye Baibulo kapena mwana wathu walephela kupanga coonadi kukhala cakecake . Cikwati ca Mwanawankhosa cidzacitika nkhondo imeneyo ikadzatha . 12 : 6 ; 13 : 28 , 29 ) Jowana ndi akazi ena ayenela kuti anali kupeleka zopeleka kuti ziziwathandiza . M’makalata ake , anachula maina awo na kuwapatsa moni . Yehova amafuna kuti uziseŵenzetsa ‘ luso la kuganiza ’ kuti udziŵe coonadi . Tinali kusangalala kwambili kuphunzitsa Baibo anthu odzicepetsa ndiponso okonda kuceleza a m’gawo losagaŵilidwa limenelo . Iye anati : “ Yehova ndiye mthandizi wanga . Sindidzaopa . Kodi ndani amene adzakhala ‘ m’magulu ankhondo ’ a kumwamba amene adzatsatila Kristu pamene akumenya nkhondo imeneyi ? Ambili anakhala ndi cidwi cimeneci cifukwa cakuti Baibo imachula za “ munda ku Edeni , cakum’mawa . ” Koma sikuti Yesu na Paulo anali kulamula atumiki kuti azikhala osakwatila iyai . Simungathe kutumikila Mulungu ndi Cuma nthawi imodzi . ” — MAT . ( Gen . 37 : 23 - 28 ; 39 : 7 - 9 , 20 - 21 ) Yosefe sanafooke iyai , kapena kuwasungila cakukhosi abale ake . Iye anali wofunitsitsa kulengeza uthenga wabwino kwa osauka , kulalikila za kumasulidwa kwa ogwidwa ukapolo ndi kumanga zilonda za anthu osweka mtima . — Yes . Tsopano , tiyeni tikambilane za mau olimbikitsa akuti , “ kuika maganizo pa zinthu za mzimu kumabweletsa . . . mtendele . ” NYIMBO : 151 , 147 Pamene mlaliki Filipo analalikila za Khristu kwa Asamariya , bungwe lolamulila linamucilikiza kwambili . Baibulo limeneli ndi losavuta kumvetsa ndi kumasulila . Pamenepo Yehova adzatidalitsa , kapena kutitsogolela pa zolinga zathu . — Miy . Pobwelela kunyumba n’takomboka kusukulu , n’nakwela pho ya malaiti . ( Yuda 14 , 15 ) Pokhala munthu wacikhulupililo , Enoki anali kuyembekezela kuti mtsogolo padziko padzakhala anthu oopa Mulungu okhaokha . — Ŵelengani Aheberi 11 : 5 , 6 . Fotokozani cocitika ca Mkristu wina amene anapeza njila zina zotumikila Yehova atapuma pa nchito . N’nadziwa kuti kugwilizana ndi anthu a Mulungu nthawi zonse kudzanithandiza kukhala wacimwemwe ndiponso kukhala m’banja labwino lauzimu . Zokamba za Satana zinadziŵika kuti zinali bodza lamkunkhuniza . Koma m’kanthawi kocepa cabe , zinthu zinasinthilatu mu umoyo wa Yobu . “ Pofuna kunithandiza , mnzanga wina ananiuza kuti niiŵaleko cabe zimene zinacitikazo . Nanga tingacite ciani tikalakwitsa ? ‘ Cikondi cimakhulupilila zinthu zonse , ’ imatelo Baibo . Mulungu akutipempha kuseŵenzetsa dzina lake . — Salimo 105 : 1 . Satana anayambitsa mafunso amene anafunika nthawi yaitali kuti ayankhidwe . Angelo a Mulungu analamula Loti kuti acoke mumzindawo ndi kukakhala ku dela la kumapili . Conco , Kazumi Minoura ndi akopotala ena anali kugwilitsila nchito makalavani opanda injini . Masiku ano , wonyamula kacola ka inkiyo akuimila Yesu Khiristu , amene akuika cizindikilo anthu amene adzapulumuka . — w16.06 , mapeji 31 - 32 . Usamadzione kuti ndiwe wanzelu . M’malo mwake amaona ena kukhala owaposa ndipo amakhala ngati wamng’ono . — Afil . Mulungu afuna kuti anthu okhulupilika amenewa “ asaonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” Kodi mukanamva bwanji poona zonsezi ? Zipatala na mankhwala sizidzafunikanso . Kodi ciyembekezo cake colimba cimakhudza bwanji maganizo na zocita zake ? Koma tifunika kusankha mogwilizana ndi maganizo a Yehova ndi zofuna zake . Masiku ano , nkhawa imabwela maka - maka pofuna ndalama ndi zinthu zofunika paumoyo . Kuphunzila za ulendowo kungatithandize kudziŵa umunthu wa Yesu , kumukonda ndi kumukhulupilila . Malemba amaonetsa bwino kuti Mikayeli ni dzina lina la Yesu Khristu . — 1 Atesalonika 4 : 16 ; Yuda 9 . ( Mateyu 6 : 8 ) Timafunika kumupempha . Ngakhale kuti njoka inaoneka ya ubwenzi , Satana Mdyelekezi anali mdani wopanda cifundo , amene anadziŵa kuti zotsatilapo zake kwa Hava zinali za imfa . TONSE timafuna kukhala na umoyo wamtendele ndi wopanda nkhawa . Kucokela nthawiyo , anthu mamiliyoni ambili afa pankhondo zina . Kodi Yehova amamva bwanji tikamavutika ? Iye adzaocha mafupa a anthu ” pa guwa la nsembe m’tauni yochedwa Beteli . ( 1 Mafumu . 10 , 11 . ( a ) Kodi mkulu angathandize bwanji m’bale amene aoneka kuti safuna kukalamila maudindo ? N’cifukwa ciani Paulo ananena kuti “ Kristu ndiye mphamvu ya Mulungu ” ? ( Maliko 14 : 7 ) Koma Yesu sanafune kuti anthuwo aike ciyembekezo cao pa zinthu zosakhalitsa . Mungawacezeleko abale okondedwa amenewa . ( a ) Kodi lemba la 2 Timoteyo 3 : 14 - 17 limakhudza bwanji acinyamata ambili masiku ano ? ( a ) Fotokozani citsanzo coonetsa kuti tifunika kuvula mwamsanga umunthu wakale . Malinga n’zimene Mau a Mulungu amakamba , mkazi wokwatiwa afunika kuvomeleza kuti mwamuna wake ndiye azimutsogolela osati makolo ake . Ise tinatumiziwa ku mpingo wa anthu akuda , umene unali na ofalitsa 14 cabe . Davide atalangidwa , anavomeleza zolakwa zake , ndipo anakhalanso paubale wabwino ndi Yehova . — Sal . Nthawi zonse pamene mubweza loni yanu , m’pamenenso amakudalilani kwambili Kodi makolo angadziŵe bwanji kuti mwana wawo angathe kudzipeleka moyenela ? Mwinanso zimene mumaganiza ndi zofanana ndi zimene ena amene tachula pamwambapa amaganiza . Ndipo cipulumutso cathu kupitila m’dipo , cimapeleka ulemu ndi ulemelelo ku dzina la Yehova . Masiku ano , na ise nthawi zina tingafunikile kupeleka ndalama zothandizila pa nchito inayake yapadela . Yehova Ndi Mulungu Wacikondi Kulandila cisomo ca Mulungu sikutanthauza cabe kupewa zaciwelewele . Kumaphatikizaponso kupewelatu zosangulutsa zolaula zilizonse . Conco , njila ina imene inu makolo mungaonetsele kuti ndinu olimba mtima komanso kuti mumadalila Yehova ndi mwa kuthandiza ana anu kudziikila zolinga zauzimu na kuzikwanilitsa . — 1 Sam . N’cifukwa ciani a Mboni sakondwelela maholide ? Nkhondo : Ufumu wa Mulungu udzacotsapo zinthu zonse zimene zimayambitsa nkhondo , monga kudzikonda , ziphuphu , mzimu wokonda dziko lako , na cipembedzo conama . Nayenso Satana adzacotsedwa . ( Sal . Paulo anapeleka moni kwa Purisika ndi Akula , ndipo anakamba kuti iye “ komanso mipingo yonse ya anthu a mitundu ina , ” anali kuwayamikila . Mwana wathu wamkazi Olga amakhala ku Estonia , ndipo kaŵili - kaŵili amanitumila foni . Anati : “ Koma woyang’anitsitsa m’lamulo langwilo limene limabweletsa ufulu , amene amalimbikila kutelo , adzakhala wosangalala policita . ” ( Yak . Pamene tikuthandiza ana athu na ophunzila Baibo kupita patsogolo , tifunika kukumbukila kuti ngati munthu sabatizika , sangakhale wotsatila weni - weni wa Khristu . Pamene Sara anali kulonga katundu , iye anavutika kusankha katundu umene adzasiya ndi umene adzatenga . Ndipo adzakhala ndi mwai woonetsa ngati amam’konda Mulungu mwa kumvela malamulo ake . 38 : 10 - 12 ) Kunena mophiphilitsa , anthu a Mulungu adzakhala “ pakatikati pa dziko lapansi , ” kutanthauza kuti adzadziŵika kuti ndi apadela . Aliyense . . . amene sanaone Moyo wanga ngati wopanda pake , kapena kulumbila mwacinyengo . ” Anthu ambili amasonkhezeledwa ndi mzimu wa dziko la Satana pankhani imeneyi . Cotelo , amadziŵanso bwino zimene timafunikila kuti tipilile . 18 , 19 . ( a ) Kodi Satana amafuna kuti tizidziona bwanji ? Pamene Yesu anali padziko lapansi , anacita zinthu zoonetsa kuti umoyo udzakhala bwino akadzayamba kulamulila . Akanakhala anzelu , akanaganizila mozama zimenezi . N’cifukwa ciani tiyenela kupewa kudzidalila ? Mwacitsanzo , katswili wina anati : “ Lamulo la Mulungu [ pa Genesis 2 : 16 , 17 ] limaonetsa kuti Mulungu yekha ndiye amadziŵa cimene cili cabwino . . . kwa anthu ndi kuti Mulungu yekha ndiye amadziŵa cimene si cabwino . . . kwa iwo . Zosangalatsa ndi zakuti abale ndi alongo ambili anadzipeleka kumuthandiza ndipo nchito imeneyi anaiona kukhala mwai wa utumiki . Yehova Ambuye Wamkulu Koposa ndiye pothaŵilapo panga . ” Tikakumana ndi vuto , tingacite ciani kuti tipewe kucita colakwa ngati cimene Yosiya anacita ? Tikamaonetsa cidwi anthu ena , io adzakhala okonzeka kumvetsela uthenga wathu , ndipo ulaliki wathu udzakhala wogwila mtima . Kwa zaka zambili , kagulu kameneka kanali na mkulu mmodzi . Koma kukalamila sikutanthauza kukhumbila mwadyela ‘ kukhala woyang’anila . ’ Kupatsa kumapindulitsadi . Mofanana ndi mmene zinalili m’nthawi ya Paulo , Akristu ambili masiku ano amapanga bajeti kapena kuika kandalama “ kenakake pambali ” kuti akaponye m’mabokosi a zopeleka za “ Nchito Yapadziko Lonse . ” ( Aroma 8 : 14 - 17 ) Nanga bwanji za anthu amene ali ndi ciyembekezo ca padziko lapansi ? Anthu anali kulidziŵa Baibulo lacigiriki la Septuagint , ndipo otsatila oyambilila a Kristu anali kuligwila mau mosavuta . Amapangitsa cilengedwe cake kucita ciliconse cimene afuna kuti akwanilitse cifunilo cake Pamene anali kuloŵa , m’bale wina anamwetulila na kukamba kuti : “ Mwacoma bwanji ? Timagwilizana ngako tsopano . ” Kuti Mkristu akhale wogwilizana ndi ena afunika kukhala wodzicepetsa . Olo kuti anali na matenda , anali wanzelu kwambili komanso anali na mtima wacikondi . Mwacitsanzo , mnzanu akuloŵa m’banja . Awa ndi amodzi a madalitso amene tapeza paumoyo wathu wonse . ” ( Agalatiya 3 : 11 ; Habakuku 2 : 4 ) Ndiye cifukwa cake tifunika kukhala ndi cikhulupililo colimba mwa Iye amene angatithandizedi . Onani zocitika izi zimene lemba la Chivumbulutso caputala 12 limanena : Cifukwa cakuti munthu sayenela kukhala m’cikondi ndi wina aliyense amene angamfikile . ( 1 Pet . 2 : 10 ) Pofotokoza colinga ca mtundu watsopano umenewu , Petulo anati : “ Inu ndinu mbadwa yosankhika , ansembe acifumu , mtundu woyela mtima , anthu a mwini wake , kotelo kuti mukalalikile zoposazo za Iye amene anakuitanani mutuluke mumdima , muloŵe kuunika kwake kodabwitsa . ” ( 1 Pet . Ngati mwapatsidwa mwayi wokamba nkhani , kodi mungaseŵenzetse bwanji mphamvu ya Mau a Mulungu pokamba nkhaniyo ? Kodi mungacite bwanji ngati akulu apanga cosankha cimene inu simunacimvetsetse kapena simunagwilizane naco ? Yesu anakana ciphuphu cacikulu koposa Mu 1979 , tinakhala na mwana wa namba 5 , dzina lake Daniel . Koma mosiyana ndi nzelu yaumulungu , ndalama sizingacititse kuti tikhale otetezeka kapena okhutila . Mwacitsanzo , Mulungu watipatsa lamulo lakuti tizipewa magazi . Pofotokoza ulosi wokhudza mapeto a nthawi ino ya zinthu , Yesu anati : “ Padzakhala zizindikilo padzuŵa , mwezi ndi nyenyezi . Padziko lapansi anthu a mitundu ina adzazunzika , ndipo adzathedwa nzelu cifukwa ca mkokomo wa nyanja ndi kuwinduka kwake . Ndani Kwenikweni Akulamulila Dzikoli ? Kaya tili m’cikwati kapena ai , kodi tingatengele bwanji citsanzo ca Paulo ? Kodi mwaona kuti ndinu ofunika kwa Yehova ? ‘ Tinalandila mzimu wocokela kwa Mulungu , kuti tidziŵe zinthu zimene Mulungu watipatsa mokoma mtima . ’ — 1 AKOR . Tsiku lina zinthu zinafika poipa . Ngati titsatila mfundo za m’Baibulo , tidzapitiliza kukonda anzathu . Monga anthu auzimu , sitifuna kucita zinthu zimene zingaononge ubwenzi wathu na Atate wathu wakumwamba . Nthawi ikakwana 12 : 00hrs , amayenda pang’ono - pang’ono kubwelela ku nyumba . Ngati timacezela anthu panthawi yoyenela kwa io , tidzatsatila citsanzo ca Paulo amene sanali ‘ kungofuna zopindulitsa iye yekha ayi , koma zopindulitsa anthu ambili , kuti apulumutsidwe . ’ — 1 Akor . Nanga n’cifukwa ciani anthu ambili sakhulupilila lonjezo limeneli ? Nayenso Bilidadi wa ku Shuwa , amene anali mnzake wa Elifazi , anakamba kuti n’zosatheka anthu kukhala olungama pamaso pa Mulungu . — Ŵelengani Yobu 25 : 4 . Komabe ndinaphunzila kuti Yehova ndi wacifundo ndi wokhululukila . Kodi sizomveka kuti Atate wathu wakumwamba amene ni waungwilo amayembekezela kuti ise tizimukonda na kumuyamikila pa zabwino zonse zimene amaticitila ? ( b ) Kodi Yehova anaonetsa bwanji maganizo ake pankhaniyi ? Jeffery wakhala akucita zamalonda ndi makampani a masitima apamadzi ocokela m’maiko a United Kingdom ndi United States . Pemphelo — Kodi Lingakuthandizeni Bwanji ? 11 Pamene musinkha - sinkha zomanga banja ndi kuyamba nchito , ganizilani ngati zosankha zanu zidzakupangitsani kuganizila kwambili zinthu zakuthupi kuposa kufuna - funa Ufumu wa Mulungu coyamba ndi cilungamo cake . N’ciani cinacititsa Yesu kukhala wacimwemwe ? ( b ) Ndi mwai wotani umene tapatsidwa ? ( Aheb . 13 : 2 ) Kupatula nthawi yoceleza ena si kutaya nthawi , ndipo n’kofunika ngako . Cifukwa Yehova ndiye mwini ciweluzo ndi cilungamo . Kodi masomphenya a Zekariya atiphunzitsa ciani masiku ano ? Kodi Yoswa analimbikitsidwa bwanji ? Anthu ambili amakumana ndi mavuto amene sitinakumanepo nao . Iye anati : “ Pamene ise a sayansi tiphunzila zinthu zodabwitsa za m’cilengedwe , nthawi zonse timaona kuti n’zadongosolo lapamwamba kwambili , cifukwa ca malamulo ake odalilika . 2 : 24 . M’madzulo mulimonse , iye anali kunyamula mtsuko paphewa lake ndi kupita ku citsime . — Genesis 24 : 11 , 15 , 16 . Nikuthokoza kwambili Yehova cifukwa ninayamba kuphunzila Baibulo na ambuya amene anali kutsutsa coonadi . ” Kuti cilango cathu ciwafike pa mtima anthu , n’ciani cimene tifunika kucita ? Mariya anatsala ku Nazareti , mwina cifukwa cakuti anali mayi wamasiye . Ili ndi funso lofunika kwambili limene wina aliyense amene anadzipeleka kwa Yehova ayenela kudzifunsa . Conco , ndinakana kusaina cikalataco . ( Mateyu 11 : 28 - 30 ) Limeneli ndi lonjezo labwino kwambili ! Kodi Mulungu anacita bwanji zimenezo ? Koma ambili , kuphatikizapo aja amene kale anali ndi khalidwe losavomelezeka ndi Mulungu koma anasintha , apitilizabe ndi khalidwe lao labwino . — Ŵelengani 1 Akorinto 6 : 9 - 11 . Yehova wandidalitsa ndi mkazi wina wokongola dzina lake Loraini Sikivou . Ngakhale kuti tinali Akatolika , ambuye anga aamuna anali osaumilila maganizo awo pa za cipembedzo , ndipo anali kulandila mabuku a cipembedzo amene anzawo anali kuwapatsa . Atangomuona mitima yao inawila moti mkwiyo wao unayaka . N’nayamba kuona monga kuti natsala pang’ono kudwala matenda ovutika maganizo . A Daka : Zikomo . Popanda Yosefe wa ku Kupuro , sembe Akhristu anapitiliza kumuopa Paulo . Mtengo wa maolivi akaudula umaphukanso cifukwa cakuti mizu yake imapita pansi kwambili ndiponso imayala malo aakulu . Yehova anasangalala kwambili pamene analenga Mwana wake wobadwa yekha . Cifukwa ca kusintha kwa kamasulidwe ka liu lakuti asher , Salimo 144 lomba imaonetsa bwino ciyembekezo cimene Davide anali naco . Ciyembekezo cakuti Mulungu akadzapulumutsa Aisiraeli kwa adani awo , adzawadalitsa mwa kuwapatsa umoyo wacimwemwe ndi waulemelelo . ( Lev . 26 : 9 , 10 ; Deut . 7 : 13 ; Sal . Inde , ngati palibe zifukwa zomveka zimene anacitila zimenezo , komiti yaciweluzo ingapangidwe cifukwa umenewo ni umboni wamphamvu woonetsa kuti anthuwo anacita ciwelewele . — 1 Akor . ( Ŵelengani Aroma 14 : 10 - 12 ; 1 Akor . 13 : 7 . ) * Kucita izi kunali koyenela , cifukwa Yesu na odzozedwa amene adzalamulila nawo pamodzi , ni amene Yehova adzawaseŵenzetsa pophwanya Satana na otsatila ake . — Aroma 16 : 20 ; Chiv . Liu lakuti “ copondapo mapazi ” limanena za dziko lino , koma limagwilitsidwanso nchito m’Malemba Aciheberi pofotokoza mophiphilitsa za kacisi wakale amene Aisiraeli anali kugwilitsila nchito . ( 1 Mbiri 28 : 2 ; Sal . Ufumu wa Mulungu wakhala ukulamulila kwa zaka zoposa 100 . N’cifukwa ciani ndi bwino tsopano kukonzekelelatu masautso ? Mtumiki wa nthambi ya m’dzikolo , dzina lake Pryce Hughes , anali munthu wokoma mtima , ndipo mwacikondi ananiphunzitsa zinthu zambili . Paulo anakamba kuti Mau a Mulungu amene Yehova watipatsa ali monga lupanga . Solomo anafunika kukhala wolimba mtima kuti akwanitse kugwila nchito imene anapatsidwa mpaka kuitsiliza . ( Sal . 136 : 15 ) Koma Mose anapulumutsidwa ndipo Mulungu anam’gwilitsila nchito kutsogolela Aisiraeli kuti apulumuke . Tikapempha Yehova kuti atithandize kupilila ciyeso , iye amatilonjeza kuti “ adzapeleka njila yopulumukila . ” Kodi dipo limakwanilitsa bwanji zimenezi ? Alendo akabwela m’mudziwo , anthu anali kucita nako nthabwala pofuna kuseketsa anzawo . Kukaca m’maŵa n’nali kucita zonse zotheka kuti nicotse maganizo olakwika amenewo . Kukhala opatsa kumabweletsa cimwemwe ngakhale tikumana ndi mavuto , ndipo Yehova amasunga lonjezo lake lakuti adzatilimbikitsa pamene tifunikila kulimbikitsidwa . “ Usagwilitse nchito dzina la Yehova Mulungu wako mosasamala . ” Koma panthawiyo , zinali zovuta kwambili kuti anthu wamba a ku England akhale na Baibo . “ Usakhale pakati pa anthu omwa vinyo kwambili , ndiponso pakati pa anthu odya nyama mosusuka . Cifukwa cidakwa ndiponso munthu wosusuka adzasauka . ” — Miyambo 23 : 20 , 21 . 10 : 8 . Ku Rwanda kunacoka lipoti lakuti : “ Anthu amene anali kuphunzila Baibulo ndi abale , sanali kupita patsogolo kwa nthawi yaitali cifukwa cakuti analibe Mabaibulo . Kodi dzina lakuti Yehova limatanthauza ciani ? Zimene anaphunzila anazikonda kwambili , ndipo mothandizidwa na Yehova analeka kucita zaciwelewele . Anakwanitsanso kuthetsa maganizo odziimba mlandu amene anali nawo . Mwacitsanzo , abale a mumpingo wanu watsopano angakhale osamasuka kweni - kweni poyelekezela na a mu mpingo wanu wakale . 24 : 15 ) Kodi panthawiyo tizidzacitilana zinthu mwacikondi ? ( Yohane 3 : 16 ) Palibe wina wapamtima pake amene akanatipatsa kuposa Yesu . Vesi imodzimodziyo ikamba kuti Inoki anapitiliza kuyenda na Yehova pambuyo pobeleka Metusela . Iye sanafunenso kukambilana nane . Atumiki a pa Beteli , amishonale ndi oyang’anila oyendela , onse amaona nchito yao kukhala yamtengo wapatali , ndiponso dalitso locokela kwa Yehova . Gulu la Mulungu limatipatsa zida zambili zotithandiza pa nchito yolalikila . Ambili mwa iwo anali na maudindo apamwamba mu ulamulilo wa Roma . Tikayang’ana zinthu zonse zimene Yehova anapanga , kaya zazing’ono kapena zazikulu , timacita cidwi ndi mmene zimaonetsela colinga cake . Yehova ananenelatu kuti masiku ano , m’dziko mudzakhala ngati muli cilala , kutanthauza kuti anthu adzakhala ndi ludzu “ lofuna kumva mau a Yehova . ” Komabe , m’Mau a Yehova muli zifukwa zomveka zotithandiza kukhulupilila kuti kucotsa munthu mumpingo ndi makonzedwe acikondi . Popeza kuti sindinawauze zimene anali kufuna , ananditumiza ku ndende ya Dzaleka , kumpoto kwa mzinda wa Lilongwe . Gwilitsilani nchito zida zofufuzila kuti mupindule kwambili ndi kulambila kwa pabanja ndi phunzilo laumwini . Ngakhale zinali conco , Petulo nthawi ina anakamba ndi kucita zinthu zolakwika . N’cimodzimodzinso aliyense wobadwa mwa mzimu . ” Kuti tidziŵe , tiyeni tiyelekezele umoyo wa Mfumu Asa ndi Mfumu Amaziya . ( Sal . 73 : 1 - 3 , 12 , 13 ) Monga kholo , mufunika kuzindikila kuti zimene mungacite na mwana wanu amene amakayikila zikhulupililo zake , zingacititse kuti cikhulupililo cake cilimbe kapena cifookeletu . Ndiyeno Mulungu anacititsa kuti mpanda wolimba wa Yeriko ugwe , ndipo Aisiraeli analanda mzindawo . Liu limeneli likupezekanso m’Mabaibulo ena a Cingelezi . ( Luka 6 : 40 ) Wofalitsa watsopanoyo , mosakaikila adzasangalala kukhala ndi munthu amene angamuthandize pakafunikila thandizo lililonse . Kuti nikwanilitse colinga cimeneci n’nafunika kumagwila nchito ya maola ocepa . Yosefe anali na manda ogobedwa muthanthwe m’munda wina wa pafupi na pamene Yesu anaphedwela . Nkhani yoopsa imeneyi inalembedwa kuti “ iticenjeze ifeyo amene mapeto a nthawi zino atifikila . ” ( 1 Akor . Cikhulupililo cimalimba ngati munthu ali na ciyembekezo . M’malomwake , iye moleza mtima anawalangiza mobwelezabweleza . Kuphunzila malemba amenewo kudzatithandiza kupindula na cisomo ca Mulungu ndi kuikabe maganizo athu pa zinthu zimene zidzatipindulitsa kwamuyaya . Nkhanizi zionetsa kuti nthawi zonse Yehova wakhala akulimbikitsa atumiki ake , ndiponso kuti kwa zaka zambili , atumiki akewo akhala akutengela citsanzo cake . Mu 1992 , ndinaikidwa kuti ndizithandizila m’Komiti ya Utumiki ya Bungwe Lolamulila . Mfundo ni yakuti , Yosefe anazindikila kuti Yehova ndiye anam’patsa mphoto na kum’dalitsa . — Gen . 2 : 10 ) Pambuyo pake , M’bale Franz ndiye anakhala wotsogolela nchito yathu . Panalibe mabuku otanthauzila mau ndi masukulu ophunzitsa cinenelo . Conco , tinaganiza zomaphunzila mau 10 kapena 20 atsopano tsiku lililonse . Nkhaniyi ifotokoza cifukwa cake tiyenela kudziŵa nthawi yabwino yokamba zinthu , zimene tiyenela kukamba , ndi mmene tiyenela kuzikambila . Tinakambilana kuti pali zosangulutsa zina zabwino , zina zoipa . Yehova ndi Mlengi wathu , ndipo amatisamalila . Timakhala acimwemwe , ndi amtendele , ndiponso timakonda Mulungu amene amatipatsa “ mphatso iliyonse yabwino ndi yangwilo . ” — Yak . Onani kuti ponena za imfa ya onse aŵili , Lazaro ndi mwana wamkazi wa Yairo , Yesu anayelekezela imfa ndi tulo . ANTHU ENA AMAKHULUPILILA kuti Ufumu wa Mulungu ni mtima wa munthu . Ena amaganiza kuti ni mtendele umene anthu adzabweletsa padziko lonse . Kodi odwazika angacite ciani kuti alimbane ndi nkhawa zimene zimakhalapo ? Komabe , pali maumboni ena amene amatipatsa cithunzi ca mmene Paulo anali kuonekela . Anali kufuna kusangalatsa Yehova ndipo anaona kuti kucita zimenezo n’kofunika kwambili kuposa nsembe iliyonse . Kodi m’Baibo muli malangizo anji pankhani ya zaumoyo ? Ndithudi , cikondi , kukhulupilika , ndi khama n’zofunika kuti banja likhale lopambana . Kukonda Yehova , Yesu , na anthu anzathu kumatilimbikitsa kulalikila ( Onani palagilafu 5 , 10 ) N’cifukwa Ciani ? 17 , 18 . ( a ) Kodi tiyenela kudzifunsa funso liti lokhudza zolinga zathu za kuuzimu ? Ndinasiya kusuta fodya . * Zosangulutsa zoyenela ni “ mphatso yocokela kwa Mulungu . ” “ Usanene kuti : “ N’cifukwa ciani kale zinthu zinali bwino kuposa masiku ano ? ” Kuti mudziŵe zambili za nchito ya makomiti 6 a Bungwe Lolamula , onani buku lakuti , Ufumu wa Mulungu Ukulamulila , pa tsamba 131 . 8 Tikhale Amodzi , Monga Mmene Yehova na Yesu Alili Amodzi Kutalitali ! — Ŵelengani Machitidwe 20 : 22 , 23 . 135 : 6 ; Yes . Yosimbiwa na Bernhard Merten ( Mac . 20 : 35 ) Mwacitsanzo , ganizilani mmene cipembedzo coona cimathandizila atumiki a Mulungu kukhala na mabanja acimwemwe . Kukhala mwana woyamba kubadwa wamwamuna unali udindo wolemekezeka , ndipo nthawi zambili iye ndiye anali kuyang’anila banja atate ake akamwalila . Pemphani Mulungu kuti amvetsele pemphelo lanu kotelo kuti mupeze mtendele pamene muvutika , ndiponso “ kuti dzina la Yehova lilengezedwe . ” — Sal . Cifukwa cakuti Mulungu ndiye anasankha Sauli kukhala mfumu ya Aisiraeli . Tonse taona kukwanilitsidwa kwa lonjezo la Yesu . ” — Ŵelengani Mateyu 6 : 33 . Mofanana ndi Yesu , timathandiza anthu kuzindikila zosoŵa zao za kuuzimu . Anthu ena amakhulupilila kuti . . . masiku otsiliza adzatha pamene dziko lapansi ndi anthu onse zidzawonongedwa . Koma ena amakhulupilila kuti zinthu zidzakhala bwino . Komabe , tingaphunzile zambili pa zocepa zimene tamva zokhudza iyeyu . Abale amene asankha kukatumikila ku maiko ena amavutika ndi zakudya zacilendo , cinenelo , miyambo , ndi zikhalidwe zosiyana ndi zimene anazoloŵela . Pamene mudzaonanso dzina la Mulungu lakuti Yehova m’Malemba Acigiriki Acikhristu kapena m’mau a munsi mu Reference Bible , mukakumbukile za Elias Hutter na Mabaibo ake a Ciheberi ocititsa cidwi . ( a ) N’cifukwa ciani tiyenela kutsatila ndandanda ya kuŵelenga Baibulo pa nyengo ya Cikumbutso ? Kuyambila pa September 1 , 2014 , kuika abale pa udindo kukucitika motele : Woyang’anila dela aliyense amapenda mosamalitsa ziyamikilo za abale a m’dela lake . Mwana akacimwa , amakhala na mlandu pamaso pa Mulungu ngati amadziŵa coyenela ndi cosayenela pamaso pa Yehova . Pamene mukulitsa luso pa nchito yanu , m’pamenenso mudzakondwela nayo kwambili . 7 , 8 . ( a ) Kodi Yehova amaganizila ciani populumutsa anthu ake pa mayeselo ? ( Mayi a Yesu ) Mateyu caputa 1 - 2 ; Luka caputa 1 - 2 ; onaninso Yohane 2 : 1 - 12 ; Machitidwe 1 : 12 - 14 ; 2 : 1 - 4 Patapita zaka , iye anapita patsogolo mwa kuuzimu , ndipo anati : “ Tsopano ndaona kuti kupempha thandizo kwa ena n’kofunika kwambili m’malo moyesa kuthetsa nekha vuto . ” Mulungu anagwilitsila nchito nsembe yake kuti mbadwa za Adamu zipindule . Nanga bwanji za anthu amene sanatumikileko Yehova ? Kodi cikhulupililo cathu cimalimbikitsidwa motani ndi zimene taphunzila pa lemba la 2 Timoteyo 2 : 19 ? Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Pamene mukuloŵa m’nyumba , pelekani moni kwa a m’banja limenelo . ” 28 : 19 , 20 ) Mwa kutengako mbali panchito imeneyi , timathandiza anzathu kucoka pamseu waukulu ndi wotakasuka wopita kucionongeko kuti abwele pamseu wopapatiza wotsogolela ku moyo . ( Mat . Mulungu wakhala akugwila nchito mosalema . Kuonjezela pamenepo , m’Baibulo mulibe malamulo acindunji onena za nchito zimene tiyenela kugwila kapena zosangulutsa zimene tiyenela kusankha . “ Kukamba mau onyoza mkazi wanu mom’pita mbali , kapena kum’kambila nthabwala zoipa , kudzapangitsa kuti ayambe kudziona kuti ni wosafunika , komanso angaleke kukudalilani , ndipo izi zingaononge cikwati canu . ” — Brian . Kodi Mulungu afuna kuti io azicita ciani ? 4 : 9 - 11 . Ndithudi , izi zionetselatu kuti Yehova amafunanso alambili ake kucita zinthu mwadongosolo . Zaka ziŵili zathunthu zinapita . Pita mu mtendele , matenda ako aakuluwo atheletu . ” — Maliko 5 : 34 . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene nsembe ya Yesu inathetsela nkhani zimene Satana anayambitsa m’munda wa Edeni . Kodi Yesu anayamba kulamulila mu 33 C.E m’njila yotani ? Koma kodi anafunikila kuyembekezela ciani ? 16 , 17 . ( a ) N’zinthu zina ziti zimene Satana na ziŵanda zake sangakwanitse kucita ? N’zoonekelatu kuti Yehova amakondwela kwambili ndi anchito odzipeleka amenewa . — Sal . Pamene Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa inapezeka mu 1947 , akatswili a Baibulo anayelekezela malemba Aciheberi Acimasorete ndi zimene zinali m’mipukutuyo . Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa inalembedwa zaka zoposa 1000 , malemba Aciheberi Acimasorete akalibe kulembedwa . M’bale Rutherford anakamba nkhani ya mutu wakuti , “ Ufumu wa kumwamba wayandikila . ” Ngati simudziŵa Malemba amene angakuthandizeni kukwanilitsa zolinga zanu , pemphani a Mboni za Yehova kuti akuthandizeni . Tidzaphunzilanso mmene cikhulupililo cingatithandizile kuona dzanja la Mulungu pa umoyo wathu . Mwacitsanzo , Akhristu ena amatsutsidwa ndi anthu a m’banja lao , ena amavutitsidwa kusukulu , ndipo ena boma limawaletsa kulalikila . Mavuto amenewo sayenela kutidabwitsa . Caciŵili , ngati aona kuti ana awo ayamba kuleka kukonda zinthu zauzimu kapena kulalikila m’gawo la cinenelo ca mpingo umene atumikilamo . John , amene anali manijala pa kampani ya nchito ya zomangamanga , ndi mkazi wake Carmen , akutumikila monga anchito odzifunila akanthawi ku Warwick . Iwo anati : “ Taona mmene Yehova watisamalila paumoyo . Mboni zoposa 8 miliyoni m’maiko oposa 230 zimaphunzitsa anthu Baibulo . Lemba la Salimo 45 limasonyezanso mmene zinthu zidzacitikila . Aaron , amene tamuchula m’nkhani yapita , anati : “ Ndimakhala wosangalala pambuyo pogwila nchito kwa maola ambili patsiku . Mkazi wake sanali Mboni , ndipo mkazi wanga anayamba kuphunzila naye Baibo . Ana amene amalangiwa mwacikondi , nthawi zambili amadzimva kukhala otetezeka . Amayi anali kuvutika posamalila ine na mlongosi wanga wamng’ono . M’bale Mumba : Mwacita bwino kundifunsa . Zinthu zosangalatsa zimene zakhala zikucitika mkati mwa zaka 100 za ulamulilo wa Ufumu zikutitsimikizila kuti Yehova akulamulila ndipo colinga cake cokhudza dziko lapansi cidzakwanilitsidwa . N’tapezeka pamisonkhano yawo kwa nthawi yoyamba , n’nasangalala ngako . Kukamba zoona , tiyeneladi kuwapemphelela mosalekeza abale amenewa . Nthambi ya ku Mexico , inatumiza kagulu ka omasulila cinenelo ca Cimaya kukakhala kudela la cineneloco , kuti azimva ndi kukamba cineneloco nthawi zonse . Nkhani ziŵilizi zidzatithandiza kuona cifukwa cake tifunika kulimbana ndi mdani wathu wamkulu ameneyu . Mavesi 5 pa mavesi 6 amenewa , anaonjezeledwa cifukwa cakuti dzina la Mulungu linapezedwanso pa Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa imene inafalitsidwa posacedwapa . Kodi mlongoyu anamvela conco cifukwa ciani ? Ndipo ndimasangalala ndikaona abale m’dziko lathu amene amaika patsogolo zinthu za kuuzimu ngakhale kuti ndi osauka . Komabe , pambuyo pophunzila Baibo , anasintha maganizo . Ungagwilitsilenso nchito cofalitsa coyenelela . Komanso waonetsa khalidwe la kuleza mtima na cilungamo pocita zinthu ndi Satana wopandukayo . Ngati muli na maganizo ena - ake olakwika ponena za Baibo , yambani mwawaika pambali kuti Mulungu akuphunzitseni . — Salimo 25 : 4 . M’malo mwake , cifuno cake cinali cakuti anthu onse asangalale ndi thanzi labwino mu Paladaiso . Cifukwa ca kusintha kwa zinthu m’gulu kumene kunacitika mu 2015 , Daniel na Miriam anauzidwa kuti azitumikila monga apainiya anthawi zonse osati apadela . ( Maliko 14 : 27 - 31 , 50 ) Koma Yesu atagwidwa , atumwi onse anamuthaŵa , kuphatikizapo Petulo . Banja lina likuyembekezela mwana . Cacikulu n’cakuti amakhala na thanzi labwino . Patapita ola limodzi , anatumilanso m’baleyo ndi kum’pempha kuti akakumane kuti akakambilane . Mu 2005 , tinabwelela kwathu ku Basalt , ku Colorado . Apanso tinali na nkhawa kwambili . Ine na Bethel tikupitiliza kucita upainiya kuno . Iye anati : “ Inde ndipita . ” — Genesis 24 : 58 . Komanso kuopa zinthu zina kumatithandiza kupewa ngozi . Koma n’kutheka kuti anaiŵalilatu zakuti anafunika kuyenda ‘ modzicepetsa ndi Mulungu wake . ’ Yoyamba , ni kuganizila za makhalidwe apamwamba a Yehova ndi ulemelelo wake . ( Yes . Posapita nthawi , mlongoyo anapita kunyumba ya munthuyo koma sanamupeze . Pali pano , “ dziko lonse ” lili m’manja mwake . Mwacitsanzo , pocilitsa munthu wolemala msana kwa zaka 18 , anati : “ Mayi , mwamasuka ku matenda anu . ” Ndipo lomba nimalalikila anthu ambili kuposa kale . ” Conco , dzifunseni kuti : ‘ Kodi ndimacita bwanji ngati m’bale kapena mlongo walakwitsa zinazake ? “ Ngakhale kuti pamalo amenewo pangapezeke anthu aŵili kapena atatu acikhulupililo cimodzi , ” mwinanso munthu mmodzi , Ambuye adzakhala pamenepo . ” Pa webusaiti imeneyi pali mbali za ana , mabanja , ndi zinthu zatsopano . Ndinafunika kusintha maganizo anga kuti ndizicita zinthu mwamtendele komanso kuona kuti ndiyo njila yabwino kwambili yokhalila ndi moyo Ngakhale n’conco , Akhristu ena amene ali pabanja asankha kupatukana ndi mnzawo pa zifukwa zina . Conco ndinayamba kukhala ndi makolo anga , ndipo ndinakondwela kwambili . Kulemekeza anthu amene afunika kupatsidwa ulemu , kumatithandiza kuti tisakhale odzikonda . Abulahamu Ndiyeno , Michael anakhala wofalitsa wosabatizika . Kodi pemphelo limatitonthoza bwanji ? Ayuda anali kudana ndi atsamunda aciroma , amene analibe nazo nchito za miyambo yawo . Koma naonso Aroma anakwimitsila zinthu Ayuda cifukwa ca nthota zawo . ” Mu caputala 12 , Paulo amatikumbutsa kuti ngakhale ziwalo zathupi zimene zimaoneka ngati n’zosafunika kapena zofooka , n’zofunika . Atumiki oyendela ena anasinthidwa kukhala apainiya apadela cifukwa ca ukalamba kapena zinthu zina . 47 : 1 - 6 ) Komabe , Aiguputo anali kuona anthu amene anali kuŵeta nkhosa kukhala osanunkha kanthu . ( Gen . Ngakhale kuti Yohane sanakambe kuti Diotirefe anali mphunzitsi wonyenga , iye anali kucita zinthu motsutsana ndi utsogoleli wa mtumwiyu . 17 : 20 , 21 ) Yesu analosela kuti kagulu kang’ono ka odzozedwa pamodzi ndi a “ nkhosa zina ” kadzakhala “ gulu limodzi . ” Cifukwa ca ici , pa miyezi 6 , tinali tinangophunzila mau ocepa cabe m’Citagalogi . Kodi anasuliza mtumiki wake amene anavutika maganizo ndi kucita mantha ? Panthawi ina , Yesu anayelekezela nchito yopanga ophunzila na nchito yofesa na kukolola mbewu . — Mat . Anthu a makhalidwe amenewa amafuna kuti ena aziwatamanda . ( Aheberi 5 : 14 ) Mkristu wofikapo amafuna ‘ kudziŵa molondola ’ coonadi ca m’Baibulo . Koma inali nthawi yakuti anthu amene anali kale Akristu amvele cenjezo la Yesu ndi kuthaŵa mu Yerusalemu . Kodi mapemphelo athu angathandize bwanji kuti tikhale ogwilizana ? ( Aroma 8 : 15 - 17 ) Popeza kuti odzozedwa adzakhala mkwatibwi wakumwamba , io akulangizidwa kuti : “ Uiwale anthu ako ndi nyumba ya bambo ako [ akuthupi ] . ” Cimatithandiza kutengela makhalidwe a Mlengi wathu Koma ise anthu opanda ungwilo , nthawi zina timalephela kukhala odziletsa . Citsanzo ca Anna cokonda Yehova cinalembedwa m’Baibo . Banja lina lacicepele ku Asia linayamikila ngako malangizo a m’Baibo . Muzithandiza ofooka . ( 2 Mbiri 16 : 9 ) Mulungu watipatsa malamulo ake kuti tipindule . Ena mwa malamulo amenewa amakhudza umoyo wabanja ndi mmene tingapezele zosoŵa zathu zakuthupi . Ngakhale kuti mlongo Etta anali kucita mbali yaikulu pa nchitoyo , iye anapeleka citsanzo cabwino pankhani yolemekeza abale amene anali kuyang’anila pa famupo . Kodi acinyamata angaonetse bwanji khalidwe labwino potenga maudindo kwa abale acikulile ? Nanga n’ciani cimene anacita ? Iye sanali kukonda mkulu wake Leya amene atate ao anapeleka kwa Yakobo kukhala ngati ndi Rakele amene Yakobo anali kufuna kukwatila poyamba . Okalamba amene anali pakati pawo anali ataonapo ulemelelo wa kacisi wa Yehova woyambilila . 2 : 10 - 12 . “ Ambili amaloŵa m’cikwati ali na ‘ maganizo ’ akuti zinthu zikadzavuta , adzasudzulana cabe . Yesu anafotokozanso za munthu wina amene anapeza cuma “ cobisika ” pogwila nchito m’munda . Yesu anadziŵa kuti ziphunzitso zake zidzagaŵanitsa anthu . Anadziŵanso kuti otsatila ake adzafunika kukhala olimba mtima kuti akhalebe okhulupilika pamene akutsutsidwa . Yehova anafuna kuti dziko lapansi lidzaze ndi ana a Adamu angwilo . Onani kuti Rabeka sanangodzipeleka kupatsa cabe madzi ngamila 10 , koma anaonetsetsa kuti ngamilazo zamwa madzi mokwanila . ( 1 Akor . 16 : 2 ) Mwezi uliwonse , mipingo imatumiza zopeleka zimenezi ku ofesi ya Mboni za Yehova imene imayang’anila dela lawo . N’cifukwa ciani muyenela kukamba zinthu mwacindunji popemphela ? Ŵelengani Aefeso 6 : 17 . YELEKEZELANI kuti ni capakati - kati pa usiku , ndipo mukuona amishonale aŵili , Paulo na Baranaba , ali m’cipinda camkati ca ndende mumzinda wa Filipi . Timadziŵa kuti kudzipatulila kwa iye ndiye cinthu canzelu kwambili cimene tinacita mu umoyo wathu . Cimodzi mwa zinthu zimene zikanawathandiza ni kukhala oceleza . Petulo anawauza kuti “ muzicelezana popanda kudandaula . ” ( 1 Pet . Kodi mtumwiyu anali kudela nkhawa kuti mwina Gayo adzaleka kuceleza alendo cifukwa coopa Diotirefe , amene anali kucotsa mumpingo Akhristu amene anali kuceleza anzawo ? Cifukwa ngati munthu sakhulupilila zimene Baibulo imaphunzitsa sangapulumuke . Komabe , io amakhulupilila kuti Mulungu amayanja anthu abwino amene ali m’zipembedzo zonse , ndipo amawaona kuti ndi alambili ake . Atumiki a Mulungu amadziŵa kuti afunika kukonda Mulungu ndi anthu ena . Kodi igwilizana bwanji na zimene zinanicitikila m’mbuyomu , zimene zikunicitikila lomba , kapena zimene zinganicitikile m’tsogolo ? ( Mateyu 18 : 12 - 14 ) Kodi tingatsatile bwanji uphungu umenewu ? Malinga ndi Ekisodo 23 : 9 , kodi Mulungu anauza anthu akale kuwaona bwanji alendo ? Nanga n’cifukwa ciani ? Kulikonse kumene ndinali kupita ndinali kukhala ndi mfuti yanga Mbali yaciŵili ya mbeu ya Abulahamu ndiyo imapanga mtundu umenewo . ( Agal . Pambuyo potumikila Mulungu kwa zaka zambili , Mkhiristu angayambe kusumika maganizo ake pa zinthu za thupi . Ndani amene angaletse kuti asabatizidwe ndi madzi ? ” — Mac . 10 : 47 . 3 : 19 ) Ngakhale n’conco , mzimu wa Mulungu umatithandiza kuti tizilalikila uthenga wabwino mwamtendele ndi mwaulemu . Iye anali kuceza kwambili na atumwi ake okhulupilika , ndipo anali kugwilizana nawo mwapadela . N’cifukwa ciani kudziŵa mwamsanga zilakolako za uchimo n’kofunika ? ( Yohane 15 : 14 ) Yesu anasankha mabwenzi ake apamtima pakati pa anthu amene anali kumutsatila mokhulupilika ndiponso amene anali kukonda Yehova ndi kum’tumikila . 2 : 8 - 14 . Pa cifukwa cimeneci , amuna ndi akazi ambili aciisiraeli anakhalanso aciwelewele . N’ndani anapeleka citsanzo copambana pa kupilila mayeselo ? Ndipo n’ciani cinam’thandiza ? Mofananamo , atumiki a pa Beteli a kumaiko a ku Europe , amene anapemphedwa kukatumikila ku ofesi ya nthambi ku Germany , naonso anamva cimodzimodzi . 24 : 13 . Ndikaukila anthu onsewo amene akukhala m’midzi yopanda mipanda ndipo alibe zotsekela ndiponso zitseko . ” Udzapita kumeneko kuti ukalande ndi kutengako zinthu zambili , ndiponso kuti ukaukile dziko loonongedwa limene tsopano mukukhala anthu . Khalani ndi Cikhulupililo Cosagwedela mu Ufumu , 10 / 15 Iye anali wofunitsitsa kugwila nchito mwakhama kuti aonetse kuti waceleza mwamuna wacikulile amene anali wacilendo . Mwa ici , tidzapewa zocitika zimene zingayambitse nkhawa . N’zoona kuti okopa Baibo analakwitsa zina poikopa . Komabe , abale ndi alongo okhulupilikawa amayesetsa kutsanzila Yehova amene afuna kuti uthenga wabwino ulalikidwe “ kudziko lililonse , fuko lililonse , cinenelo ciliconse , ndi mtundu uliwonse . ” Iye amakondwela akakumbukila cinthu cimodzi coonetsa kukoma mtima cimene cinam’thandiza kuti ayambe kulambila koona . — 2 Akor . Cimeneci ndico ubatizo . ” — 1 PET . M’nyuzipepalayi , mkulu wacipembedzo wina anam’funsa ngati anthu amene anafa asanaphunzile za Yesu ali m’moto ku helo . ( 2 Sam . 15 : 31 ) Mofananamo , masiku ano anthu ampatuko ndi ena amene amayambitsa magaŵano mumpingo , amakamba “ mau okopa ndi acinyengo , ” n’colinga cakuti azioneka ngati acikondi , pamene colinga cawo ceni - ceni n’cadyela . — Aroma 16 : 17 , 18 . Ndi ciyambi cotani cimene Mulungu anapeleka kwa amuna ndi akazi ? Iye anakamba kuti : “ Akawalala anathyola nyumba yathu na kuba katundu wanga wambili . Pa colinga ciliconse cimene mwalemba , citani zotsatilazi : Mauwa anali kusonyeza cikondi ndi ulemu . — The International Standard Bible Encyclopedia . 20 : 6 . 34 : 10 ) Mose anali mneneli wapadela kwambili . Conco , Lefèvre analeka kuphunzila ziphunzitso za anthu . Iye anaika maganizo ake onse pa nchito yomasulila Baibo . Anthu ambili safuna kuuzidwa zocita ndi wina aliyense . “ Makutu ako adzamva mau kumbuyo kwako , akuti : ‘ Njila ndi iyi . ’ ” — YES . M’nkhani ino , tidzakambilana mfundo zina za m’buku la Levitiko , zimene zidzatithandiza kuphunzila miyezo ya Mulungu ya ciyelo , ndi mmene tingaigwilitsile nchito paumoyo wathu . ( 1 Atesalonika 2 : 13 ) Tambani kavidiyo kakafupi kakuti Kodi Tingatsimikizile Bwanji Kuti Baibulo Limakamba Zoona ? Tili na zifukwa zomveka zokhulupilila kuti akufa adzauka . Koma pa cifukwa cina , safuna kudzipeleka kwa Yehova na kubatizika . Kukhala na cikhulupililo cakuti akufa adzauka kunam’thandiza kukhalabe wolimba . Lolani Mau a Mulungu kukutsogolelani . Kodi izi zitanthauza kuti tizingodela nkhawa “ pa nkhani ya zovala ” ? Kodi mau a pa 1 Petulo 5 : 10 agwilizana bwanji na zimene zinacitikila Nowa , Danieli , na Yobu ? Ngakhale kuti onse , Nowa ndi ana ake atatu , aliyense anali na mkazi mmodzi , anthu anali kukwatila cipali m’nthawi imeneyo Cikhiristu cisanayambe . Kumayambililo kwa zaka za m’nthawi ya atumwi , Ufumu wa Roma unali kulamulila kuyambila ku Britain kufika ku Gaul , ( imene tsopano ni dziko la France ) mpaka kukafikanso ku Egypt . Taganizilani zitsanzo zina za amene anakumanapo ndi zimenezi . “ Pitilizani kulolelana ndi kukhululukilana ndi mtima wonse . ” — Akolose 3 : 13 . Kodi Mumaona “ Wosaonekayo ” ? Ponena za “ masiku otsiliza , ” Baibulo limati : “ Anthu oipa ndi onyenga adzaipilaipilabe . ” Oyang’anila dela ambili amakamba kuti iwo na azikazi awo amalimbikitsiwa ngako akalandila kakalata kowayamikila pambuyo pocezela mpingo . AMAI ANGA anandifunsa kuti : “ N’cifukwa ciani sulambilako mizimu ya makolo athu ? Timaseŵenza kuti tipeze zofunika pa umoyo ndi kuti tizicita bwino utumiki wathu . ( July 1 , 2013 ) ndi yakuti “ N’cifukwa Ciani Mulungu Amalola Kuti Anthufe Tizivutika ? ” ( Luka 22 : 20 ) Yesu ndiye Mkhalapakati wa pangano limeneli , ndipo odzozedwa okhulupilika a m’pangano limeneli amapatsidwa coloŵa ca kumwamba . — Aheb . Maganizo anga onse anali pa maseŵela basi . Cifukwa cakuti kukhala paubwenzi ndi Mulungu ndiye colinga cacikulu cimene tingakhale naco pa umoyo wathu . Ndinadziyeletsanso mwakuthupi . Zinaoneka ngati kuti moyo ndi tsogolo la Mose zinali m’dzanja la Farao . Sara , na onse amene amatengela cikhulupililo cake , akuyembekezela kudzasangalala kwamuyaya . — Yohane 5 : 28 , 29 . Nkhani yotsatila idzationetsa mmene tingakhalilebe odzicepetsa panthawi zovuta . Timapeza njila yothandizila ena “ Pembedzelo la munthu wolungama limagwila nchito mwamphamvu kwambili . ” — Yakobo 5 : 16 . Mwacitsanzo , pangano la ukwati lomwe linali pakati pa Abulahamu , Hagara ndi Sara , linali kuimila pangano la Yehova ndi mtundu wa Isiraeli komanso mbali yakumwamba ya gulu la Mulungu . ( Agal . 2 : 18 ) Yakobo anaonetsanso kusiyana pakati pa kungokhulupilila zinthu ndi kuonetsa cikhulupililo . Ngati timadziganizila kuposa mmene tiyenela kudziganizila , tingayambe kucepetsa colakwaco , kuimba mlandu ena , kapena kukana kuti ndife tacita . Yehova satikakamiza kuti tizim’konda ndi kum’tumikila . ( Ezara 8 : 24 - 34 ) M’nthawi ya atumwi , Paulo analandila ndalama zimene Akhristu anapeleka kuti zikathandizile abale a ku Yudeya . Mwacitsanzo , n’cinthu canzelu kuti mwamuna na mkazi akangoyamba cibwenzi adziikile malile oyenela pa nkhani yoonetsana cikondi . Iye anapempha Mulungu katatu kuti amucotsele “ munga m’thupi . ” Yesu anadziŵa kuti malonjezo a Mulungu salephela . Ndithudi , kumeneko kudzakhala “ kuuka kwabwino kwambili ” poyelekezela na kuuka kwa anthu akale . Udindo wa bwanamkubwayo unali kutengela Aroma misonkho kwa anthu na kukhazikitsa mtendele ndi dongosolo . ( Yak . 1 : 19 ) Kenako yelekezelani kuti ndinuyo , ndipo dzifunseni kuti : ‘ Ndikanakhala kuti ndine , kodi ndikanamva bwanji ? Kaya cifukwa cake cikhale cotani , tizikumbukila amene amafuna kutifooketsa . Mafanizo ena atatu ndi okhudza kapolo wokhulupilika ndi wanzelu , anamwali 10 , ndi nkhosa ndi mbuzi . Bungwe la akulu limapenda mosamala nkhaniyo kuti lidziŵe ngati komiti yaciweluzo ifunika kupangidwa . Mose na Yeremiya , nawonso anadzikayikila pamene Yehova anawapatsa utumiki watsopano . ( Eks . Tsopano Yosefe ali ndi zaka 28 , ndipo wakhala m’ndende pafupifupi zaka 10 . M’citundu coyambilila , mau akuti ‘ kukhulupilila pambuyo pokhutila , ’ amatanthauza “ kukhala wosakayikila kuti zinazake n’zoona . ” Ndimadziŵa kuti ndagwiladi nchito tsiku limenelo . ” — Nick . CIYEMBEKEZO 16 : 32 ) Iye anali “ wofatsa . ” Koma tikusangalala cifukwa cakuti anali kudziŵa “ njila ” yopitila ku malo kumene adzakhala kwamuyaya . 28 : 6 , 7 ; 29 : 10 - 12 , 18 . 12 , 13 . ( a ) Kodi Mboni za Yehova zimati bwanji pankhani yosankha zosangulutsa ? Nanga ndi mfundo ziti za m’Baibulo zimene tingatsatile ? 15 : 24 ) Koma tsopano monga Mfumu yaulemelelo , iye adzalamulila dziko lonse lapansi . Izi n’zimenenso zinacitika na Ciheberi komanso Cigiriki , zinenelo zimene zinagwilitsidwa nchito polemba Baibo . Anthu m’dzikoli amaona kuti kupsa mtima kuli cabe bwino , koma vuto n’lakuti kumanyozetsa Mlengi wathu . Popeza kuti nthawiyo cipali cinali cofala , mwina Sara anaganiza kuti n’zimene mwamuna wake ayenela kucita . “ Mulungu , amene amalimbikitsa osautsika mtima , anatilimbikitsa . ” — 2 AKORINTO 7 : 6 . ( Agal . 2 : 20 , 21 ) Muzikhulupilila kuti kupyolela m’dipo limeneli , macimo anu angakhululukidwe . 3 MUZIPEMPHELA NTHAWI ZONSE . 3 : 10 ) Yehova analonjeza kuti munthu wopatsa mowoloŵa manja adzalandila mphoto . N’zinthu ziti zimene zimayambitsa “ nsautso m’thupi ” ? Mulungu sayankha mapemphelo a anthu amene samumvela . Alongo , okwatiwa ndi osakwatiwa omwe , amakhala na cimwemwe coculuka ngati auzako ena uthenga wabwino monga anchito anzake a Mulungu . ( 1 Ates . 1 : 2 , 3 ) Iye anawauzanso kuti azilimbikitsana wina na mnzake . Anati : “ Pitilizani kutonthozana ndi kulimbikitsana . ” — 1 Ates . Ngati ndi conco , mumapemphela pa zinthu ziti ? Tate wina ku Brazil anati : “ Timatengeka ndi Kulambila kwa Pabanja cakuti ngati sindinakumbutse banja kuti nthawi yatha timafika mpaka pakati pausiku . ” Koma tinali kukondwela tikaona mmene anthu anali ofunitsitsa kulidziŵa bwino gulu la Yehova . ANTHU ambili amaloweza pamtima Pemphelo la Ambuye . Mabungwe onse oipa adzaloŵedwa m’malo na boma limodzi la Ufumu wa Mulungu , labwino ndi logwilizana . Nthawi imeneyo idzakhala yokondweletsa ngako . Kucotsa munthu wocimwa mumpingo kungamuthandize kuzindikila chimo lake . TSAMBA 9 • NYIMBO : 45 , 70 Malinga na Bungwe lochedwa International Labour Organization , anthu 21 miliyoni amuna , akazi , ndi ana , amagwilabe nchito monga akapolo . Taganizilani zocita za Manase mfumu imene inacita zinthu zoipa kwambili kuposa Ahabu . Tiyenela kukhala ndi maganizo ngati amene mtumwi Paulo anali nao , pamene anati : “ Sitikubwelela m’mbuyo . ” — 2 Akorinto 4 : 1 , 16 . Kapena Baibulo limanenanso kuti zaka 1,000 zikadzatha , Satana adzamasulidwa kuphompho , ndipo “ adzatuluka kukasoceletsa mitundu ya anthu kumakona onse anayi a dziko lapansi . Mitunduyo ndiyo Gogi ndi Magogi , ndipo adzaisonkhanitsa pamodzi kunkhondo . ” ( Chiv . N’tafika kumeneko , n’napatsa mkulu wa asilikaliyo pepala limene n’nalembapo kuti , “ Nifuna cabe kukhala msilikali wa Khristu . ” Kodi ndimayesetsa kukhala ndi diso lolunjika pa zinthu za kuuzimu ? ’ Pamene Mose anauza Yehova kuti anali kuopa kuti anthu sadzam’khulupilila , Mulungu anam’konzekeletsa ndi zimene zinali kubwela . ( Sal . 94 : 19 ) Yehova wakhala akunithandiza pa mavuto a m’banja , citsutso , zolefula , na nkhawa . Akatswili aonetsa kuti anthu ofika m’mahandiledi miliyoni anafa ndi nthomba m’zaka za m’ma 1900 . Tingaonetse bwanji kuti timayamikila mwayi wathu wokhala anthu a Yehova ? Yehova amafuna kuti amuna azicita umutu wao mwacikondi Akapeza kuti munthuyo anacitadi chimo , ayenela kuweluza mlanduwo mogwilizana ndi Malemba . 1 : 4 , 5 . Tingasinkhesinkhe mwapemphelo za ciyembekezo cimene Mulungu watipatsa . — 1 / 15 , masamba 14 - 16 . ( Luka 10 : 7 ) Koma ngati taona kuti sitidzapita pa zifukwa zina zomveka , tingaonetse kuti timawakonda na kuwaganizila amene anatiitanawo mwa kuwadziŵitsa mwamsanga za kusinthako . Kodi mzimu wa dziko wokonda cuma watiyambukila ? Umaonetsanso kuti kucita cifunilo cake ndiye cinthu cofunika kwambili pa umoyo wanu . Lonjezo limeneli ndi nkhani yaikulu . Ndipo , kwa anthu a ku Korea , Shim Cheong ndi citsanzo cabwino ca mwana wodzipeleka . M’mabanja mudzakhala mulibe cikondi cacibadwa , ana sadzamvela makolo awo . Mtumwi Petulo anaticenjeza kuti : “ Mdani wanu Mdyerekezi akuyendayenda uku ndi uku ngati mkango wobangula , wofunitsitsa kuti umeze winawake . ” — 1 Pet . Cifukwa ca mantha , abale ena aleka kugwilizana na mpingo . M’dela limenelo , nthawi zambili timakumana ndi anthu otsutsa uthenga wathu . N’cifukwa ciani acicepele ambili amasangalala na nchito yopanga ophunzila ? Kodi n’ciani cingathandize kuti mwana wosamalila makolo asatope ? Pamene Satana anapandukila ulamulilo wa Mulungu , iye anasonkhezela makolo athu oyamba kuti naonso apanduke . Mwacitsanzo , pofuna kutonthoza mwana , makolo ena amapatsa mwanayo ciliconse cimene wafuna . M’bale wina wa kumeneko , dzina lake Vasile , anati : “ Anthu a kuno amalemekeza Baibo , amakonda cilungamo , ali na mabanja ogwilizana , komanso amayesetsa kuthandizana . ” Kukhala munthu wauzimu kungatithandize kukhala na umoyo wacimwemwe ndi wokhutilitsa . Kukhulupilika kwanu monga mkulu kunali kukondweletsa Yehova , monga mmene inunso kunali kukukondweletsani . — Miy . Koma anthu inu simunafune zimenezo . ” — Mateyu 23 : 37 . Nanga anthu amene ali ndi ciyembekezo cokhala padziko lapansi ali ndi udindo wotani ? N’zoona kuti timakonda Yehova , ndipo sitifuna kukhala wodzikonda ndi woipa monga Abineri ndi Abisalomu . Kwenikweni , kulanga ndi kupeleka malangizo , kuphunzitsa , ndi kuongolela . Ifenso ticite cimodzimodzi poyesetsa kukhala ‘ omvela mocokela pansi pa mtima . ’ 10 : 44 , 45 ) Conco , kuyambila nthawi imeneyo , anthu akunja osadulidwa anayamba kupatsidwa mwai wokhala Isiraeli wa kuuzimu . Kodi ise tifunika kucita ciani na makonzedwe a umutu amene Mulungu anakonza ? Pafupi - fupi 100 zimaononga manyumba , ndipo civomezi cimodzi camphamvu kwambili cimacitika caka ciliconse . Ndipo iwo amazindikila zimenezo ! ” ( Onani nkhani yakuti “ Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi ” m’magazini ino . ) ( Ŵelengani 1 Petulo 4 : 10 ) Kodi mpingo umapindula bwanji ? Tifunika kukhalabe chelu na zinthu zimene zingacititse kuti tileke kukonda Ufumu . Zina mwa zinthu zimenezi ndi kukonda zinthu zakuthupi ndi cilakolako coipa ca kugonana . ( Miy . 4 : 23 ; Mat . Ndinali kufuna kuti banja lathu likhalenso pamtendele , ndipo ndinaganiza kuti ndikamvela makolo anga naonso adzandimvetsela . Yehova watipatsa ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha . Wolemba Salimo 102 anavutika maganizo . Zimam’pweteka mtima akaona kuti tikukonda kwambili munthu wina kapena cinthu cina ciliconse kuposa iye . Tingapemphele pa zinthu zotsatilazi : Koma sindinalionepo . ” ​ — YUMIKO , JAPAN . ( Yak . 2 : 15 , 16 ) Mofananamo , kukonda Yehova ndi anansi athu kumatilimbikitsa kugwila nchito yolalikila mwakhama , osati kungopempha Mulungu ‘ kuti atumize anchito okakolola . ’ — Mat . Mwacitsanzo , ena amakamba kuti Kolosase Mfumu ya ku Lydia , anatumiza mphatso zamtengo wapatali kwa wansembe wina wolosela zam’tsogolo ku Greece m’tauni ya Delphi , kuti adziŵe ngati adzapambana pa nkhondo yolimbana na Koresi wa ku Perisiya . Ndidzatsanulilanso mzimu wanga pa anchito anu aamuna ndi aakazi . ” Anthu anga amene anafa adzadzuka ndi kuimilila . . . . Mbewu imene inagwela pa nthaka yabwino inazika mizu , inamela , kenako inakula n’kukhala mmela wa tiligu . Baibo imalangiza Akhiristu eni - eni kuti : “ Musaiŵale kuceleza alendo . ” ( Aheb . ( b ) Kodi amuna Acikristu ayenela kucita bwanji zinthu ndi akazi ao ? Tikakumana ndi mayeselo aakulu , sitiyenela kukaikila kuti Mulungu amaona mavuto athu , ndi kuti adzatithandiza cifukwa ndife amtengo wapatali kwa iye . — Sal . Zosankha zathu pa umoyo zifunika kuonetsa kuti tili na maganizo monga a Petulo , amene anauza Yesu kuti : “ Ambuye , inunso mukudziŵa kuti ndimakukondani kwambili . ” Nkhalango . Komabe , madela onse aŵili anachedwa Meriba cifukwa ca mikangano imene inacitika kumeneko . — Onani mapu 7 , pa peji 38 , m’kabuku kakuti Buku Lothandiza Pophunzila Mau a Mulungu . Cioneka kuti Yesu anali kukamba nsomba zimene zinali capafupi kapena bizinesi ya nsomba imene Petulo anali kucita . A Inoki : Ndakondwela kukumana nanu a Yohane . Iye anali kumva mau a abale ake akuzimililika pang’onopang’ono ali m’citsime ndipo anali kuona cabe kathambo kozungulila . ( Mat . 19 : 27 ) Yesu sanam’dzudzule Petulo cifukwa ca funso limeneli . Dikishonale ina inafotokoza kuti ; zolakwa zimabuka cifukwa ca “ kuganiza molakwika , kusadziŵa zonse , kapena kusamvetsela . ” Ndikhulupilila kuti mukuvomeleza kuti kuitana padzina la Yehova n’kofunika kuti tikapulumuke , ndipo Yesu anadziŵa bwino zimenezi . Kungayambitsenso matenda a ciwindi na kalambalala . Pamenepo , ndinayamba kuphunzila za Mulungu woona , Yehova . Khoti Lalikulu la Ayuda linali kumuzonda Yesu . Kuciyambi kwa kabuku kameneko , iye analemba zinthu zomvetsa cisoni , koma zimene analemba posacedwapa , zinali zabwino ndi zokondweletsa . ( 1 Pet . 2 : 9 , 10 ) — 11 / 15 , tsamba 24 - 25 . Koma timakhulupilila kuti Mlengi wathu adzatipatsa zinthu zimene tifunikiladi panthawi yoyenela ndipo m’njila yoyenela , monga mmene tate wacikondi amacitila . — Luka 11 : 11 - 13 . Iye anati : “ Ndinali kuŵelenga nkhani za anthu amene anali kupemphela kwa Mulungu kuti awatumizile munthu owaphunzitsa za iye . Koma ngati palibe , udzabwelela kwa inu . ” Mwai wodziŵika ndi dzina la Mulungu umafuna kucita zambili . Mnyamata wina , dzina lake Austin anati : “ N’nali na mtima wosafuna kumvela . Koma makolo anga anali kunipatsa malamulo amene ningakwanitse kuwatsatila , anali kunifotokozela cifukwa cake anipatsa malamulowo , na kumakamba nane momasuka . Cilamulo cinateteza Aisiraeli kuti asatengele mitundu yoyandikana nao imene inali kukonda ciwelewele ndi kulambila mafano . Monga tinakambila m’nkhani yapita , Baibo siichula msinkhu umene munthu afunika kufikapo kuti ayenelele kubatizika . Popeza kuti Yehova amatidziŵa bwino kwambili , amadziŵanso bwino zimene timafunikila kuti tipilile Iwo ndi otsimikiza mtima kutumikila Yehova mokhulupilika cifukwa cakuti amam’konda , ndi kukondanso Mwana wake , ndipo amatelo osati cifukwa cakuti mapeto ali pafupi . ( Oweruza 2 : 1 - 3 , 11 - 15 ; Salimo 106 : 40 - 43 ) Mwacionekele , zinali zovuta kuti mabanja amene anali kukonda Yehova akhalebe okhulupilika kwa Iye m’zaka zovuta zimenezo . Atumiki ambili a Mulungu adzionela okha kuti ukacimwa umapeza mpumulo ngati wapempha na kulandila thandizo kwa akulu . 149 : 4 ; Aroma 5 : 3 , 4 ; Akol . 3 : 15 ) M’bale Ulf , amene watumikila mu utumiki wa nthawi zonse kwa zaka 45 , anati : “ Nimalema ngako nikagwila nchito yolalikila , koma nchitoyi imanithandiza kukhala wokhutila komanso kuona kuti umoyo wanga uli na phindu . ” Olo kuti palibe maikolofoni , mau a mkambiyo akumveka mu holo yonseyo , cakuti anthu akumvetsela mwachelu nkhaniyo kwa ola limodzi na hafu . Baibulo limatithandizanso kupewa ciwelewele mwa kutiuza mmene tifunika kucitila zinthu ndi anthu amene si amuna kapena akazi anzathu . Ponyamuka mumzinda wa New York , pa ulendo wake wacinayi , M’bale Russell anakwela sitima yapamadzi yochedwa Mauretania . Kodi tiyenela kudzifunsa ciani ? N’cifukwa cake Paulo anakamba kuti uthenga wabwino “ unalalikidwa m’cilengedwe conse ca pansi pa thambo . ” ( Akol . Mavuto amene Danieli anakumana nawo . ( Ŵelengani Genesis 12 : 14 - 20 . ) Timalalikila kwa anthu osiyanasiyana . ( b ) Yesu anacita ciani Filipo atam’pempha kuti aonane ndi anthuwo ? Ngati okwatilana salemekezana , angayambe kukamba mokalipilana , monyozana , komanso mopeputsana . Ocita kafuku - fuku amakamba kuti makhalidwe amenewa ni cizindikilo cakuti akhoza kudzasudzulana m’tsogolo . Inde , iye anayesetsa kupititsa patsogolo kulambila koona . — 2 Mbiri 14 : 4 . Mkazi wake , yemwe ni wolimba mwauzimu , sanali kuvutika kuyankha mafunso a mwamunayo . Koma Robert nthawi zambili anali kukangiwa kuyankha mafunso a mkazi wake , ndipo anali kucita manyazi . Kucokela nthawiyo , Baibo yakhala ikusintha umoyo wanga . ( Yes . 54 : 17 ) Sitimamuopa Satana ndi anthu ake . Akaona kuti Mulungu wayankha mapemphelo awo cikhulupililo cawo cinali kulimba . ( Neh . 1 : 4 , 11 ; Sal . Lemba la 2 Akorinto 12 : 1 - 4 ( Ŵelengani . ) limafotokoza za masomphenya amene Paulo anaona . 16 “ Anthu Ofatsa Adzalandila Dziko Lapansi ” Mauwa akuonetsa kuti akazi amenewa anali kugwililidwa . N’cifukwa ciani anthu a Mulungu afunika kupewa ngozi ? Kodi sitiyenela kuwayamikila na kuwalimbikitsa ? M’caka ca 1961 , n’nauzidwa kuti nizitumikila mu Ofesi ya Wosunga Cuma , imene inali kuyang’anilidwa ndi m’bale Grant Suiter . Pitilizani kulalikila mokangalika , ndipo musaleke kuona kuti nchito yopulumutsa moyo imeneyi ni yofunika ngako . Baibo imati : “ Munthu wosonyeza kukoma mtima kosatha amapindulitsa moyo wake , koma munthu wankhanza amacititsa kuti thupi lake linyanyalidwe . ” Mmenemo tidzakhala ndi nchito zambili zokondweletsa . Koma ngakhale pali pano , pali nchito yofunika ngako , yolalikila uthenga wabwino ndi kupanga ophunzila . Timadziwa kuti Baibulo ndi locokela kwa Mulungu cifukwa limanena molondola zinthu zimene zidzacitika mtsogolo . Kwa zaka zambili , nchito yolalikila sinali kugwilidwa mwakhama . ( 1 Sam . 16 : 7 ; Maliko 2 : 8 ) Nanga bwanji tikamalankhula kapena kupemphela mokweza mau ? N’cifukwa ciani nkhani ya m’Baibo ya Davide na Goliyati ni yoona ? Pali pano , nikhala mumzinda wa Belgorod , ndipo abale kuno amanithandiza kwambili . Khalanibe Auzimu Potumikila Mumpingo wa Cinenelo Cina , Oct . Rose anabatizika mu 2009 , ndipo m’caka cotsatila , anayamba upainiya wanthawi zonse . ( Luka 8 : 1 - 3 ) Pa Pentekosite wa mu 33 C.E . , amuna ndi akazi pafupifupi 120 analandila mzimu wa Mulungu mwanjila yapadela . Ngati ticita zimenezo , tidzalimbitsa cikhulupililo cathu ndi ca ena . Komabe , Yehova Mulungu anadziŵa kuti mbali imeneyi inali ulosi woonetsa kuti Mesiya sadzaphwanyidwa fupa lililonse akadzaphedwa mwa kupacikidwa pamtengo wozunzikilapo . — Salimo 34 : 20 ; Yohane 19 : 31 - 33 , 36 . Timaona umboni wa zimenezi pakagwa tsoka . Ndipo iye amatipempha kuti timuyandikile . Yesani kuzindikila zimene sakanakwanitsa kucita , ndi zimene anakwanitsa kucita . Koma kodi Aroma caputa 8 imakamba cabe za odzozedwa , kapena imakhudzanso Akhiristu oyembekezela kudzakhala padziko lapansi ? Aisiraeli sanaganizile za mavuto amene angabwele cifukwa cosamvela Mulungu . Caka na caka , kumacitika zivomezi zazikulu pafupi - fupi 50,000 zimene zimakhudza anthu . N’cifukwa cake amakonda kutamanda anthu ena mopambanitsa m’malo mowapatsa ulemu woyenelela . Atamva mau a m’Cilamuloco , Yosiya anaona kuti afunika kucita zinthu zina zambili kuti akwanilitse cifunilo ca Mulungu . A Zulu : Ndikuona kuti inunso mumalikhulupilila Baibulo . Ndiponso , Yakobo 1 : 17 limakamba kuti Yehova “ sasintha ngati kusuntha kwa mthunzi . ” ( Yoh . 5 : 43 ) Conco , mukadzakumana ndi otsutsa mu ulaliki , mudzakhale olimba mtima . 21 Kuitaniwa Kucoka mu Mdima Masiku ano , sitingakhulupilile zonse zimene taŵelenga kapena kuona pa Intaneti . Pambuyo pake anawalimbikitsa ndi mau akuti : “ Musacite mantha . N’cifukwa ciani Yesu anakamba fanizo la mwana wolowelela ? Zingakhalenso zosavuta kugonja ku ciyeso ngati tili na nkhawa kapena ngati ndise osungulumwa . Kuti tiyankhe funsoli , tiyeni tikambilane za mavutowo . Ni cocitika citi cimene Yesu anauza ophunzila ake kukumbukila ? Masiku ano , nikutumikilabe monga mkulu mumpingo , olo kuti n’nadwalapo sitroko kaŵili konse . Colinga cacikulu cimene Yehova anauzila anthu kulemba cigawo cimeneci ca Baibo , cinali cakuti adziŵikitse Mesiya na kutsogolela anthu ake kwa iye . ( b ) Kodi Paulo anaonetsa bwanji kuti anali kuona ulaliki kukhala wofunika ? Anthu a mumzindawo anafuna kuti agwile azondiwo , koma Rahabi anawabisa padenga la nyumba yake . Koma masiku ano n’kololeka kukamba za madalitso amene anthu a Mulungu ali nao . Nthawi zina Mulungu anali kulankhula ndi anthu amene analemba Baibulo kupyolela mwa angelo , m’masomphenya ndi m’maloto . Yosimbidwa ndi Anthony Morris III Koma kodi cikhulupililo n’ciani kweni - kweni ? 3 : 3 , 4 . Ngati n’conco , dziŵani kuti Yehova angakuthandizeni ngati mumulola kutelo . Koma mtsikanayo anali pa cisumbali ndi m’busa wacinyamata , ndipo anaumilila kunena kuti afunitsitsa kukhala ndi mnyamatayo . M’nkhani ino , tikambilana zitsanzo za m’Baibulo zimene zingatithandize . ( 2 Pet . 3 : 13 ) Ngati sitiika maganizo athu pa zinthu zakumwamba , tingaone monga kuti malonjezo akucedwa kukwanilitsika . Ndipo zingacititse kuti tibwelele m’mbuyo kuuzimu . Ndipo sindinali kumwetulila ngakhale pang’ono . Yehova Mulungu , amene anapeleka mphatso ya dipo yopulumutsa moyo , afuna kuti mum’dziŵe bwino . Afunanso kuti mukhale naye paubale . Ndiyeno , pokamba nkhaniyo , seŵenzetsani malemba oyenelela amene munasankha . Pezani njila zingawathandize kuganiza , koma zogwilizana na msinkhu wawo . Conco , tingacite bwino kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ine nimalimbikitsa abale na alongo kukhalabe okhulupilika kwa Yehova ? Baibulo limati : “ Kwenikweni , iye sali kutali ndi aliyense wa ife . ” M’mbili ya makono ya Mboni za Yehova , aja amene akutsogolela nchito yolalikila amacita khama kulalikila ndi kuphunzitsa uthenga wabwino padziko lonse . Nthawi zina , kucita zimenezi kungakhale kovuta . Nanga anthu ena tingawathandize bwanji kupeza mtendele ? Wolamulila wake adzasamalila bwino anthu . — Ŵelengani Yesaya 11 : 4 ; Danieli 2 : 44 . Olo kuti Yesu anavutika kwambili akalibe kufa , sanali kukhala wacisoni kwambili . Kenako , Mfumu yatsopanoyo inayamba kuyenga , kuphunzitsa , ndi kulinganiza atumiki ake padziko lapansi kuti acite cifunilo ca Mulungu . Atate wacifundo m’fanizo ili akuimila Atate wathu wakumwamba Yehova , yemwe ndi wacikondi . Koma anthu ena pafupifupi 1,000 anauzidwa kubwelela cifukwa cosoŵa malo okhala . MFUMU yaulemelelo yakwela pa hachi cifukwa ca coonadi ndi cilungamo ndipo ikupita kukagonjetsa adani ake . Yehova amadziŵa kuti Satana wacititsa khungu anthu osakhulupilila . ( 1 Pet . 5 : 1 ) N’cimodzi - modzi ndi makomiti 6 a Bungwe Lolamulila . ( Luka 21 : 16 , 17 ) Anafunika kulimbana ndi anthu osakhulupilika , aneneli onyenga , ndi kuonjezeka kwa kusamvela malamulo . Akhristu a ku Antiokeya wa ku Siriya a m’zaka 100 zoyambilila , anakumana ndi zinthu zimene zinayesa kudzicepetsa kwawo ndi mtima wawo wokhululukila ena . Kodi tsopano tidzakambilana ciani ? M’nthawi ya kukhalapo kwa Kristu , Akristu odzozedwa akamaliza moyo wao wa padziko lapansi amaukitsidwila ku moyo wakumwamba . N’tayamikila mlongo wina amene anapeleka yankho , abale na alongo amene anakhala kumbuyo kwake anayamba kunipatsa zizindikilo zoonetsa kuti yankho limene mlongoyo anapeleka silinali lolondola . Conco , mwamsanga n’nalata m’bale wina kuti ayankhenso . Ndikugwila mwamphamvu ndi dzanja langa lamanja lacilungamo . ” N’naona kuti nifunika kupitiliza kuyesa - yesa kuti nisinthe . 3 : 27 , 28 ; 1 Yoh . 3 : 17 . Makolo , ngati ana anu akuvutika kujaila mu mpingo watsopano , muzipemphela nawo pamodzi za nkhaniyo . ( Deuteronomo 32 : 4 , 5 ) Baibulo limanena kuti pali wina wake woipa amene akulamulila dzikoli . — Ŵelengani 1 Yohane 5 : 19 . Na ise masiku ano cingatitengele nthawi kuti ticotse tsankho mumtima mwathu . Anapayanso ana ake onse 10 mwa kucititsa “ cimphepo ” cimene cinagwetsa nyumba imene munali anawo . Izi n’zimene Yesu anatanthauza pamene anauza ophunzila ake kuti akhale “ asodzi a anthu . ” Kodi ‘ imfa , mdani wotsilizila , idzaonongedwa ’ motani ? ( Gen . 1 : 27 , 28 ) Conco , iye ayenela kuti anadziŵa kuti kugonana pakati pa anthu na ziwanda n’kulakwa komanso n’kosagwilizana ndi cilengedwe . Mmishonale wina , dzina lake Kim , anati : “ Mbali ina m’gawo lathu , anthu ambili anakumana na mavuto aakulu cifukwa ca nkhondo moti anatayikilidwa katundu wawo yense . Anali kuyenda mu mzinda na mzinda kukalalikila uthenga wabwino wokamba za Ufumu wa Mulungu . Iwo akayambana ndi mnzawo wa m’cikwati , amangomuthaŵa . Yosiya Magazi amenewo anacititsanso kuti macimo akhululukidwe kosatha . Limatiuza kuti winawake amamvetsela mapemphelo amene amapelekedwa m’njila yoyenela , ndi opempha zinthu zoyenela . Koma iye sanamvele uphungu wa Mulungu . Makolo afunika kumvetsela ana ao akamalankhula kuti awadziŵe bwino . Kampuyo inali pafupi ndi mzinda wa Véroia , umene m’nthawi za m’Baibo unali kuchedwa Bereya . Koma pamene Mulungu anawathandiza kumvetsetsa tanthauzo la malembawo , iwo anasintha maganizo olakwikawo . Pali mamapu oonetsa malo a m’Baibo amene angakuthandizeni kudziŵa malo ochulidwa m’Baibo ndi kumvetsetsa nkhani zimene muŵelenga . Kodi anthu ake opanda ungwilo amawaona bwanji ? Iye ali moyo ndipo akutsogolela pa nchito imene imakhudza munthu aliyense padziko lapansi . 26 : 24 - 26 ) Akulu angathandize anthu aconco kuona kuti kukhumudwa , cizondi , ndi kusungila ena cakukhosi , ni makhalidwe amene safunika m’gulu la Mulungu . Pofuna kukumbutsa ocotsedwa zimene angacite kuti abwelele kwa Yehova , nthawi ndi nthawi akulu amayendela anthu ocotsedwa amene aonetsa mtima wolapa . Iye anacitilidwa zinthu zoipa kwambili komanso zopanda cilungamo . Kodi zisiyana bwanji ? “ Zinthu zimene timafunikila ” ni zinthu zimene munthu afunika kukhala nazo kuti akhale ndi moyo . Zimene amacita zimapindulitsa aliyense . Tikamatsatila malamulo amenewa timakhala acimwemwe , ndipo koposa zonse cikhulupililo cathu mwa Yehova cimalimba kwambili . — Tito 1 : 13 . Didier amaseka akakumbukila nthawi imene anayamba kuphunzila Cimalagase . Ndiyeno tingam’fotokozele kuti imfa sinakhalepo kumwamba kucokela paciyambi . Imfa ili cabe pano padziko lapansi . 1 : 26 ; 2 : 19 , 20 ) Mulungu sanalenge anthu angwilo mamiliyoni ambili kuti adzaze dziko lapansi . Musamakayikile kuti Yehova anakukhululukilani ( Onani palagilafu 14 - 16 ) Muziwayamikila pa khama lawo lophunzila citundu canu . Kugwila nchito yolalikila ndi wina kumakupatsani mwai ‘ wopitiliza . . . kulimbikitsana ’ mosasamala kanthu za mmene ulaliki wanu ulili pa tsikulo . — 1 Ates . Zoonadi , Yehova anakhala Mfumu pa mtundu watsopanowo . Ndiyeno , Yehova anafunsa Mose kuti : “ Kodi adzayamba liti kundikhulupilila ? ” N’zinthu ziti zimene Mkhristu angafunike kuleka kuti Mulungu apitilize kumucitila cifundo ? Pa Pentekosite mu 33 C.E . , Akhiristu okhala mu Yerusalemu analandila Akhiristu atsopano ocokela kumalo osiyana - siyana . Nanga n’cifukwa ciani n’zocititsa cidwi kuti iye anakwanitsa kuwapilila ? Ndipo ngati tinalembedwa nchito ndi Mkristu mnzathu , timapewa kumudyela masuku pamutu mwa kufuna kuti aziticitila zinthu zina zabwino kuposa anchito ena . N’cifukwa ciani Baibulo la Dziko Latsopano analikonzanso ? ( b ) N’ciani cimene acinyamata angaphunzile pa zimene Yesu anali kucita ali wacinyamata ? “ Kwa Adamu , Mulungu ananena kuti : ‘ Cifukwa . . . wadya cipatso ca mtengo umene ndinakulamula kuti usadzadye , . . . Udzadya cakudya kucokela m’thukuta la nkhope yako mpaka utabwelela kunthaka , pakuti n’kumene unatengedwa . ( Luka 21 : 24 ) Conco tinganene kuti kusokonezedwa kwa ulamulilo wa Mulungu kunali kudakalipo pamene Yesu anali padziko lapansi ndipo kunayenela kupitilizabe mpaka m’masiku otsiliza . Conco , tingathe kuona kuti Mulungu anaipanga mwanzelu kwambili Baibo . Pamene Ufumu wa Roma unapeleka lamulo lakuti anthu akalembetse m’kaundula , Yosefe ndi Mariya analabadila . Iye sanapemphe Mulungu kumupatsa zida zambili zankhondo . Nyanja Yofiila 1513 B.C.E . Yesu aukitsidwa 33 C.E . ( Aroma 13 : 1 - 7 ) Cifukwa cakuti tapanga Yehova kukhala Ambuye wathu Wamkulu Koposa . ( Luka 4 : 43 ) Ndiye cifukwa cake kale kunali Akristu amene anali kuchedwa “ atumwi . ” Liu limeneli limatanthauza anthu amene atumidwa kuti akacite cina cake . ( Ezara 3 : 1 , 2 ) Iwo anali okondwa ngako , ndipo zinali kuoneka monga kuti palibe cimene cikanawafooketsa . Lidzakhalabe lolimba mosasamala kanthu za kukhumudwitsana , matenda , mavuto a zacuma , kapena kuvutana ndi acibale . Koma ngakhale tili m’malo otetezeka mwauzimu , zilakolako zoipa zikhoza kuzika mizu m’mitima yathu . Timacita zilizonse zimene tingathe kuti tipewe zinthu zimene zingacititse imfa . Iye anati , “ Pamene mwana wanga wamkazi anandiuza kuti anali ndi cibwenzi ku sukulu , poyamba ndinakalipa kwambili . Mfundo imeneyi imagwilanso nchito pa zinthu zamtsogolo zimene afuna kudziŵa . ( Luka 10 : 2 ) Mau a Yesu amenewa , amene anakambidwa zaka pafu - pifupi 2,000 zapitazo akufotokoza bwino mmene zinthu zilili ku Myanmar masiku ano . Zocitika za m’Baibo zimene takambilana zatithandiza kuona kuti ciukililo n’cotheka . ( Chiv . 7 : 9 ) Mosasamala kanthu za citundu cathu , kapena kumene tikhala , tingaonetse kuwala kwathu “ monga zounikila m’dzikoli . ” — Afil . Nanga iye amaiona bwanji nchito yolalikila ? Masiku ano , anthu ambili amaona kuti cikwati ndiponso kukhala wokhulupilika m’cikwati n’kwacikale ndipo n’kosatheka . 15 : 32 - 38 ; 20 : 29 - 34 ; Maliko 1 : 40 - 42 . Kuwonjezela apo , Lefèvre anawonetsa poyela maganizo olakwika a anthu amene anali kutsutsa kuti Baibo imasulidwe m’Cifulenchi . M’malomwake , Yehova adzatidalitsa cifukwa coyesetsa kukhalabe oyela m’dziko loipali . Ndipo pokamba na Mariya , anayamba mwa kupeleka moni . Zaka zambili pambuyo pake , Satana ataponyedwa pansi kucoka kumwamba , anapitilizabe kuneneza atumiki okhulupilika a Mulungu . Paulo analembela Akhiristu anzake odzozedwa kuti : “ [ Yehova ] anatilanditsa ku ulamulilo wa mdima , n’kutisamutsila mu ufumu wa Mwana wake wokondedwa . Mwa Mwana wakeyo , tinamasulidwa ndi dipo , kutanthauza kuti macimo athu anakhululukidwa . ” ( Akol . Koma kuti akakhale na umoyo umenewo pali zimene anafunika kucita . A Zulu : N’zoona zimenezo . M’kupita kwanthawi , anthu ambili sanali kukambanso Cigiriki na Cilatini . Nanga zimaimila ciani ? Mtima wake unali kukondwela mwa Yehova . — 1 Sam . 2 : 1 , 2 ; ŵelengani Masalimo 61 : 1 , 5 , 8 . Mtumwi Paulo anafotokoza zina mwa nkhanizo . 10 : 23 ) Tikuyembekezela mwacidwi nthawi imene anthu onse adzagonjela kuulamulilo wa Yehova . 6 : 15 , Buku Lopatulika . Mulungu Amakonda Anthu Okhulupilika , Apr . Ungaphwanye zinthu . ” Koma masiku ano , zinthu ndi zosiyana ndi mmene zinalili anthu ali angwilo . 15 : 35 - 38 ; 17 : 27 . Ndinali kudziŵa kuti Baibulo ndiponso mzimu woyela wa Yehova n’zimene zingathandize munthu kusintha maganizo ake ndi kuyamba kumvetsetsa coonadi . Kodi sizolimbikitsa kuganizila nthawi pamene anthu onse okhulupilika adzakhala angwilo ? Koma , kukhala ndi cikhulupililo ceniceni sikutanthauza kudziŵa cabe zinthu zinazake zokhudza Mulungu . Ganizilani zimene zinacitikila wolemba Salimo 73 . Anthu aconco ayenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ndimangofuna kupititsa patsogolo zofuna zanga kapena ndimafuna kusamalila nkhosa za Yehova modzicepetsa ? ’ Ganizilani cabe cisoni cimene mzimayiyo anakhala naco ! Makolo anzelu amene ali ndi mabanja ogaŵanika , amacita zilizonse zimene angathe kuti akondweletse ana ao ndi ana opeza kuti aliyense azidzimva kuti ndi wokondedwa ndipo anadalitsidwa ndi mphatso yapadela ndi kuti aliyense akusangalala m’banja . — Aroma 2 : 11 . Nanga bwanji za milandu ya kupha munthu mwangozi ? Kodi Jowana anathandiza bwanji pa utumiki wa Yesu ? Nanga tingaphunzilepo ciani pa citsanzo cake ? ndi yakuti “ Kodi Nkhosazo ndi Mbuzizo Zili ndi Mtsogolo Motani ? ” 1 : 22 ) Ife tonse tidzapindula mwa kudziŵa mmene Mulungu amaonela okalamba . Ganizilani mmene Satana akanasangalalila sembe Sara anaganiza zosiya Abulahamu na kukhala mkazi wa Farao . Kodi umenewu si umboni wamphamvu wotsimikizila kuti malonjezo ena onse a Yehova adzakwanilitsidwa ? — Yos . Nkhaniyo imapitiliza kuti : “ Kwa io maloto amenewo ndi mau akewo cinakhala cifukwa cinanso comudela . ” Nthawi zambili amacita zimenezi kupitila mwa abale ndi alongo athu , kuti ‘ tikhale olimba mtima ndithu ndi kukamba kuti : ‘ Yehova ndiye mthandizi wanga . Sindidzaopa . Komabe , tingacite bwino kudzifunsa kuti , ‘ Kodi nthawi zonse nimaonetsa cikondi ceni - ceni , osati cadyela kapena cacinyengo ? ’ ( Aheberi 5 : 14 ; 6 : 1 ) Munthu amene amakhala ndi nthawi yocepa yosinkhasinkha za Mulungu , pang’nopang’ono angayambe kutaya ubwenzi wake ndi Yehova kapena angafike pomusiilatu . Tingatengele kulimba mtima kwake , kugwila nchito kwake mwakhama , kuceleza alendo , ndi kudzicepetsa kwake . Munthu wa m’fanizoli anali ndi matalente 8 , cimene cinali cuma cambili panthawiyo . Mudzadziŵa zabwino ndi zoipa . ” Abale na alongo ambili amene atumikila Yehova kwa nthawi yaitali , amakonda kukamba kuti masiku ano kuli cakudya cauzimu ca mwana alilenji kuposa kale lonse . Tsopano tiyeni tikambilane za Gidiyoni ndi kuona mmene tingatengele citsanzo cake cabwino . Iye anali kukonda kukhala woyamba mumpingo , sanali kulandila mwaulemu ciliconse cocokela kwa Yohane , ndiponso anali kunenela zamwano mtumwiyu ndi Akhristu ena . Kodi kupeleka ulemu woyenelela kwa ena kumatithandiza bwanji ? 2 , 3 . Anati : “ Pamene tinabwelela ku mpingo wa Cifulenci , mwana wathu anapita patsogolo kuuzimu ndipo anabatizika . Mwacionekele , makolo ake aciiguputo , aphunzitsi , ndi alangizi anali kumulimbikitsa kukhala na zolinga zimenezi . Kodi akazi okhulupilika aonetsa bwanji kukhulupilika kwao kwa Yehova pa nthawi yovuta ? Patapita zaka 27 kucokela pa Pentekosite mu 33 C.E . , zinaonekelatu kuti “ coonadi ca uthenga wabwino ” cinalalikidwa kwa Ayuda , ndi anthu a mitundu ina “ m’cilengedwe conse ca pansi pa thambo . ” — Akol . ( a ) Tingakambitsilane bwanji ndi munthu amene amakhulupilila kuti anthu onse abwino amapita kumwamba ? Ndipo pamene tilambila Mulungu na mtima wonse , timakhala na cimwemwe codzaza tsaya . Ndi citsanzo cotani cimene mtumwi Paulo anapeleka coonetsa cifukwa cake Akristu sayenela kutengamo mbali m’mikangano ya m’dzikoli ? “ Ndidzasinkhasinkha za nchito zanu zonse . ” — SAL . “ Makolo anga amaona kuti ndine wodalilika pamene nigwila nchito za pakhomo popanda kukumbutsidwa nthawi na nthawi . ( Yesaya 55 : 8 , 9 ) Atumiki ake amaona kuti kutengela makhalidwe a Yehova n’kofunika kwambili . N’zoonekelatu kuti Satana amafunitsitsa kutilepheletsa kukhala okhulupilika kwa Mulungu . Mwacitsanzo , safotokoza mfundo zambili zokhudza zovala zimene Akhristu angavale . Ine ndinali kutumikila m’Dipatimenti ya Utumiki , ndipo Susan anali kutumikila kocapila zovala . Conco , m’malo mopatsa mkazi wanga adresi yake , iye ndiye anatenga yathu . N’cifukwa ciani Abulahamu anali wokonzeka kuyembekezela Yehova ? Nanga ni madalitso anji amene iye adzalandila cifukwa ca kuleza mtima kwake ? Pakati pa zitsanzo zabwino za anthu amene anayamikila colowa cao ca kuuzimu , sitingalephele kuchula Mwana wa Mulungu , Yesu . Uthenga wa m’Baibo unamfika pamtima cakuti anatsimikiza mtima kusintha khalidwe lake . Kodi anthu ambili amakonda kusangalala ndi zinthu zotani ? Tili ndi cikhulupililo cosagwedela cakuti Ufumu wa Mesiya ndiwo njila yokha imene Mulungu adzagwilitsila nchito kukwanilitsa cifunilo cake ca dziko lapansi ndi ca mtundu wa anthu . — Chiv . Kumeneko ndiye kwawo kwa anthu a mtundu wa Antandiroyi . Kodi Yehova anamvela bwanji ? ( b ) N’cifukwa ciani sitifunika kucita zaciwawa olo pamene ena akuticitila zinthu zopanda cilungamo ? Nanga bwanji ngati tsiku lina mulibe mwai wokhala ndi Baibulo ? Kuti tidziŵe mmene Yehova amaonela zinthu tiyenela kuŵelenga ndi kuphunzila Baibulo nthawi zonse Ndipo pali madalitso oculuka kwambili amene tikuyembekezela , ndipo sitingathe kuwaona onse m’maganizo mwathu . ( Mat . ( Ŵelengani Yohane 10 : 16 . ) Panthawiyo , apainiya anali kupeleka maola 100 pa mwezi . Kuti ana anu azimasuka nanu , io ayenela kudziŵa kuti mudzawapatsa mpata wokamba nao ndi kuti ndinu ofikilika . “ Tsopano nikhulupilila kuti Baibulo imene nili nayo ni mphatso yocokela kwa Mulungu ” Mwacitsanzo , ufumu wa Mulungu utatsala pang’ono kukhazikitsidwa kumwamba , gulu la Akristu odzozedwa linali lotangwanika kutumikila Mulungu . Ndipo ndikhulupilila kuti inunso mudziŵa kuti kungonena kuti ndimakhulupilila Mulungu ndi Yesu si kokwanila . Nanga tingapeze mapindu anji ngati tiyesetsa kukhala mwamtendele ndi anthu onse ? Ambili amakamba mofanana ndi mmene mlongo wina analembela kuti : “ Baibulo lili monga thumba lokhala ndi zinthu za mtengo wapatali . Lomba onse aŵili amakhulupilila Mulungu maningi , na kumvetsetsa colinga cake cokhudza anthu cofotokozedwa m’Baibo . Zikuoneka kuti pa anthu 60 miliyoni amene anali kukhala mu ufumu wa Aroma , anthu oposa 4 miliyoni anali Ayuda . Paulo anachula “ ciphunzitso cokhudza . . . kuuka kwa akufa , ” monga mbali ya “ ciphunzitso coyambilila ca Khristu . ” ( Aheb . Pofika kumapeto kwa zaka za m’ma 1970 , m’madela ambili , nchito yophika cakudya pamisonkhano inapeputsidwa . Malemba amakamba kuti odwala khate afunika kukhala “ kunja kwa msasa ” . Koma olemba Talmud ena anamasulila mawu amenewa kuti odwala khate afunika kukhala kunja kwa mzinda . Anthu akakhala pafupi naye anali kufunika kukhala chelu kuti asawavulaze . Saganizila zofuna za ena . Cifukwa cakuti timakhulupilila Atate wathu wakumwamba ndi kuitanila pa dzina lake , iye amatisamalila ndi kutiteteza . Sikuti ni anthu ocepa cabe amene adzapindula ndi madalitso a Yehova iyayi . Yesu anati : “ Aliyense wocita cifunilo ca Mulungu , ameneyo ndiye m’bale wanga , mlongo wanga ndi mayi anga . ” Nanga panakhala zotulukapo zotani ? Ahabu atamva ciweluzo cimene Yehova anapeleka , “ anang’amba zovala zake n’kuvala ciguduli . Iye anayamba kusala kudya , kugona paciguduli ndipo anali kuyenda mwacisoni . ” 7 , 8 . ( a ) Kodi Solomo anaononga bwanji colowa cake cakuuzimu ? Kukamba zoona , nkhawa ndiyo inali copinga cacikulu cimene n’nafunika kulimbana naco . ” Ngakhale kuti ophunzilawo anazunzidwa , io anagwilitsila nchito bwino nthawi ya mtendele mwa kulalikila uthenga wabwino kulikonse . — Ŵelengani Aroma 12 : 18 - 21 . Koma makolo awo anaona kuti kusamuka sikukanawathandiza kukhala pa ubwenzi wabwino na Yehova . ( Yohane 11 : 18 ) Kutatsala milungu yocepa Yesu asanamwalile , m’mudzi umenewu munacitika cinthu cina comvetsa cisoni . ( Sal . 25 : 14 ) Mulungu amam’konda . ( Yohane 17 : 3 ) Ngati wina wakuuzani kuti pamene munali mwana , munthu wina anapulumutsa moyo wanu , mudzakhala ndi cidwi cofuna kudziŵa zambili zokhudza munthuyo , komanso cifukwa cake anakupulumutsani , si conco ? ( Miy . 13 : 10 ) Ndipo cacitatu , zikadziŵika poyela kuti tinacita zinthu modzigangila ( m’mphamvu zathu ) , tikhoza kucititsidwa manyazi kapena kudzitonzetsa . Mose anali mkhalapakati wa pangano la Cilamulo , koma Yesu ndiye Mkhalapakati wa pangano latsopano . Tikulakalaka nthawi imene anthu onse adzalemekeza dzina la Yehova . 5 : 1 - 11 ) Koma kuona mtima kumaloŵetsamo zambili . Baibulo limati : “ Anatsegulilatu maganizo ao kuti amvetse tanthauzo la Malemba . ” — Luka 24 : 45 . Ndipo amathandiza ndi kutonthoza odwala ndi okalamba cifukwa cokonda zabwino . Kuonjezela apo , “ onse ofuna kukhala ndi moyo wodzipeleka kwa Mulungu mwa Kristu Yesu , naonso adzazunzidwa . ” — 2 Tim . Mayankho anu pa mafunsowa angakuthandizeni kuona ngati mumam’dziŵa bwino Yehova kapena ayi . Cocitika cimeneci cimagwilizanitsa anthu ambili - mbili pa dziko lonse lapansi caka ciliconse . Yehova ndiye anatilenga ndipo tifunika kumumvela . Motelo , wofedwa kapena wofeledwa sayenela kudziimba mlandu ngati wasankha kukwatilanso kapena kukwatiwanso . Koma amayesetsa kuona zabwino mwa ife . Conco , kucotsa munthu mumpingo kumathandiza anthu ena kudziŵa kuti anthu a Yehova ndi oyela ndipo amayesetsa kutsatila malangizo a m’Malemba kuti akhalebe oyela . Iye ni Atate wathu , Mulungu wathu , ndi Bwenzi lathu ! — Sal . N’cifukwa ciani muli oyamikila malangizo a pa Aroma caputa 8 ? Mukamavomeleza zolakwa zanu , ana anu adzakulemekezani 5 : 19 ) Conco , tiyeni tikhalebe maso ndi kukumbukila kuti mapeto a dzikoli ali pafupi kwambili . Ngati tiyesetsa kucita zambili pa kulambila kwathu , timaonetsa kuti timakonda Yehova ndipo tinadzipelekadi kwa iye . Zoona n’zakuti . . . Timoteyo anali na cikhulupililo colimba . Mulungu analosela kuti posacedwapa zinthu padzikoli zidzasintha kwambili . ( Mac . 24 : 10 , 15 , 24 , 25 ) Koma pamene Paulo anakamba kuti kuuka kwa akufa ni mbali ya ciphunzitso coyambilila , kapena kuti “ mfundo zoyambilila za m’mau opatulika a Mulungu , ” sanatanthauze kuti ciphunzitso ca kuuka kwa akufa n’cosafunika kweni - kweni . ( Aheb . M’kupita kwa nthawi , Sadiq anakhala mlaliki wacangu wa uthenga wabwino . Baibulo limafotokoza kuti Satana ndi “ wolamulila wa dzikoli ” osati Mulungu . Ndipo limati “ dziko lonse lili m’manja mwa woipayo . ” Iye anatumikila Mulungu mokhulupilika kwa zaka zambili , ndipo Yehova anali kum’cilikiza . ( Yesaya 40 : 29 ) N’zoonekelatu kuti Yehova akanafuna , akanacititsa kuti tisamavutike ngakhale pang’ono polimbana ndi zofooka zathu . ( Mateyu 24 : 14 ) Buku la m’Baibo la Danieli , limatiuza kuti Ufumu umenewu ni Boma la Mulungu . ( Mat . 10 : 5 - 7 ) Ngakhale kuti Filipo anali wotangwanika ndi ulaliki , anapatula nthawi yophunzitsa ana ake akazi anayi kulalikila mogwila mtima coonadi ca m’Baibulo . ( Mac . Ndingatsimikize bwanji kuti Yehova Mulungu amandiŵelengela ? Tsiku linafika lakuti Kingsley akambe nkhani mu Nyumba ya Ufumu . ( b ) Ni malangizo ati opita kwa makolo amene ali pa Deuteronomo 6 : 5 - 7 ? Faizal amene takamba m’nkhani yoyambilila , anaganiza zophunzila Baibulo n’colinga cakuti adzionele yekha ngati n’locokeladi kwa Mulungu . Yehova sanalenge anthu ndi ufulu wakuti azidzilamulila okha popanda citsogozo cake . M’malo moŵelenga malemba ambili , tingangosumika maganizo pa mau a Chivumbulutso 21 : 4 . Muyenela kukhala okoma mtima m’zokamba na zocita zanu . Zimenezi zinacitika akalibe kutulukila makina opulintila . M’bale Mumba : Koma kodi munthu angasonyeze bwanji kuti amakhulupililadi Mulungu ndi Yesu ? Ndiyeno , inafotokoza zimene kholo lacikhristu lingacite pothandiza mwana wawo amene wayamba kukayikila zimene amakhulupilila . M’masomphenya a namba 6 a Zekariya taphunzila kuti anthu okonda Yehova safunika kuba mwanjila ina iliyonse kapena kulumbila mwacinyengo . 5 : 33 ) Kodi mwamuna angacite ciani kuti mkazi wake azim’lemekeza maningi ? Kucoka panthawi imene ndinabatizidwa , ndakumana ndi zinthu zambili zimene zikanandipangitsa kucita ciwawa . Yehova anauza Adamu mosapita mbali mfundo imeneyi ngakhale Hava asanalengedwe . Citsanzo cacitatu ndi cokhudza ulaliki wa pafoni . Mayi wina ku South America dzina lake Sabina , anaona kuti mfundo za m’Baibo n’zothandiza . Kwa Mulungu , limenelo ndilo banja . Ndolo zanga ! Zibangili zanga ! Zimenezi zimakonzekeletsa abalewo kuti adzakwanitse kutumikila bwino monga abusa a “ gulu la nkhosa za Mulungu . ” — 1 Pet . M’zaka zaposacedwapa , Yehova watipatsa zofalitsa zambili zokhudza acinyamata . ( 2 Mbiri 35 : 23 , 25 ) Koma m’Baibo mulibe mau oonetsa kuti anacita zimenezo . Atate ake anati , “ iye amalimbikitsidwa ndi Kulambila kwa Pabanja , ndipo zimenezo zimam’cititsa kuti azisangalala . ” Nanga timapindula motani ? Mtumwi Paulo anafotokoza kuti mbali za Cilamulo zinali m’thunzi wa ‘ zinthu zabwino zimene zinali kubwela . ’ — Aheb . Kayendedwe ka zinthu kameneka sikaima , kamacitika nthawi zonse . Dzinali ndi lacilendo kwambili . ’ ” — Zenon wa ku Ontario , Canada . Ndipo imawapatsa nthawi yambili yocita nchito yao yofunika kwambili ya upainiya , imene ndi kusodza anthu . “ Tikhoza kupeleka malangizo kwa mwana mobweleza - bweleza n’kuyamba kukaikila ngati iye amasungadi zimene timamuuza . Koma tsiku limene tidzalephela kucita zimene timakamba , iye adzatiuza kuti sitinacite zimene timamuuza . * ( Ŵelengani 1 Akorinto 15 : 50 - 53 . ) 12 Muziyamikila Mphatso Yanu ya Ufulu Wosankha Zocita Kodi adzaopa Yehova ndi kuzindikila ubwino wotsatila miyezo ya Mulungu ? Conco , munthu afunika kubatizika kuti akhale Mboni , olo kuti m’mbuyomo anabatizikapo ku cipembedzo cina . — Ŵelengani Machitidwe 19 : 3 - 5 . 20 : 8 , 9 . Ucimo wa Adamu unakhudza bwanji mbadwa zake ? Kupita patsogolo kocititsa cidwi kumeneku ndi kogwilizana ndi cifuno ca Yehova cakuti “ anthu kaya akhale a mtundu wotani , apulumuke ndi kukhala odziŵa coonadi molondola . ” Apainiya aŵili akugaŵila kapepa kauthenga kwa munthu wopita na njila ku Freetown , likulu la dzikolo , m’nyengo ya mvula Tidzaphunzila ciani m’nkhani yotsatila ? Conco , anthu anzelu apaulendo anali kugona kwa anzawo , ndipo Akhristu anali kugona kwa Akhristu anzawo . ( Onani cithunzi - thunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Kodi anthu atatu okwela pa akavalo amene akutsatila Yesu amaimila ciani ? Kodi Akhristu afunika kuuona bwanji ufulu ? Koma tiyenela kupempha Yehova kuti atithandize . Ni nkhani yokondweletsa , ndipo ni mbali yofunika kwambili ya ‘ uthenga wabwino wa Ufumu . ’ Mwacitsanzo , pamene Mfumu Hezekiya anali pafupi kufa , Yehova anamucilitsa . Conco , n’nayamba kukonda Mulungu ndi kumuopa . Ataona kuti ni wokonzeka , anamulimbikitsa kucita zimenezo . Ndiponso ngati ena mumpingo adziŵa za vuto lanu , angakulimbikitseni . ( 1 Petulo 2 : 22 ) Cifukwa cakuti Yesu anali wangwilo , iye sanalandile cilango ca imfa ndipo akanakhala ndi moyo kosatha monga munthu . 3 : 18 ) Kodi Yehova anadalitsa khama la Eduardo ? Ndiyeno Yehova , Atate wathu , adzakhala “ zinthu zonse kwa aliyense . ” — 1 Akor . 19 , 20 . ( a ) Kodi ciyembekezo canu cingakwanilitsidwe bwanji ? Nkhaniyi idzatilimbikitsa kuyamikila kwambili zimene Ufumu wa Mesiya wakwanilitsa pa zaka 100 zoyambilila . Kodi Yesu akanaonadi kuti kuziponya pansi kucoka pamwamba pa kacisi n’ciyeso ? 6 : 1 ) Mwina tsankholo linayamba cifukwa ca kusiyana kwa zinenelo . M’kupita kwa nthawi , yankho lake lakhala loonekela bwino . Khalani Wodzicepetsa ndi Wacifundo Monga Yesu Mphamvu ya Imfa Imfa si nkhani yosangalatsa . Paulo anali kum’konda kwambili Timoteyo . Iye anali kum’patsa malangizo othandiza kwambili . Ndikali kamtsikana , ndinali ndi cikhulupililo colimba mwa Mulungu . 18 : 18 ) N’ciani cinathandiza Davide kukhalabe wodzicepetsa ? Tingaonetse kuti timayamikila kwambili Yehova ndi zinthu zimene amatipatsa mwa kukonzekela misonkhano ndi kutengamo mbali mokwanila . — Sal . Kuti mucite zimenezi , mwina mungafunike kucepetsa zinthu zina zosafunika kweni - kweni zimene mumacita . ( Aroma 5 : 12 ) “ Munthu mmodzi ” ameneyo ni Adamu . 17 , 18 . ( a ) Kodi Satana angatipangitse bwanji kuvula cisoti cathu ? ( Yobu 6 : 24 ) Ndiponso sitiyenela kuulula nkhani zacinsinsi zimene ena sayenela kumva . ( Aheb . 13 : 8 ) Popeza kuti “ Mtumiki Wamkulu wa moyo ” amadziŵa mmene cisoni cimaŵaŵila , “ amatha kuthandiza anthu amene akuyesedwa . ” ( Mac . Buku lina limati , “ Ophunzila a Yesu anali kuona kuti imfa ndi tulo , ndipo manda ndi malo opumulila . . anthu amene anafa ali ndi cikhulupililo . ” * — Encyclopedia of Religion and Ethics . Anali kukonda kunipatsa nchito zambili monga kukwela m’mitengo kuti nidule nthambi zake ndipo n’nali kusangalala pocita zimenezo . Kodi ise amene tidzakhala m’Paradaiso kwamuyaya tili “ ngati akufa ku ucimo ” m’lingalilo lanji ? M’mau ena anthu ena amaona kuti Baibo inathelatu nchito . Apo n’kuti n’nali n’tainyamula mfuti yanga . Amanenanso za nthawi pamene anthu abwino adzamanga nyumba zao - zao , adzalima minda ndi kulela ana m’mikhalidwe yabwino . Koma moyo wathu uli na colinga capadela , cimene munthu akacidziŵa , amakhala na cimwemwe cokhalitsa . Ngati titsatila ndondomeko ya Yehova , timaonetsa kukhulupilila lonjelo lake lakuti adzaticilitsa na kutikhululukila . ( Deut . 32 : 29 ) Kupyolela m’Baibulo , Mulungu woona amatiuza za njila yabwino . Amatiuzanso mapindu amene timapeza tikatsatila njilayo , ndi zotsatilapo zake tikatenga njila yoipa . Ngati munasonyeza kudzipeleka kwanu kwa Mulungu mwa ubatizo wa m’madzi posacedwapa , mosakaikila mudzapindula ndi thandizo locokela kwa ena amene akhala akulalikila kwa nthawi yaitali kuposa inu . 2 : 18 , 19 . N’ciani cinacitika kwa anthu a Mulungu atumwi atamwalila ? Zim’vuta kumvetsa mmene munthu angakhalile alibe ciyambi . Mulungu sangacite zimenezo . Amayi ake anabwelela mumpingo , ndipo iye ni wokondwela ngako kuti akutumikilanso nawo pamodzi . “ N’nacita mantha kwambili n’taŵelenga koyamba za amuna anayi okwela pa mahosi . Yelekezelani kuti mukuona magaleta anayi , okonzekeletsedwa bwino kaamba ka nkhondo , akuthamanga “ kucokela pakati pa mapili aŵili . . . amkuwa . ” Nchito yapadela imeneyi ‘ ikuchukitsa Yehova , ndipo ni cizindikilo coti sicidzacotsedwa mpaka kalekale . ’ ( Yes . Ndi zifukwa ziti zimene zimaticititsa kukhulupilila kuti mapeto adzafika nthawi iliyonse ? * — 1 Akor . Mwacitsanzo , ganizilani za abale aŵili ocokela m’banja limodzi amene anali kutumikila kutali ndi makolo ao . Kodi mumapemphela kuti mupeze phunzilo la Baibo ? [ Bokosi papeji 5 ] “ Nkhondo Kumwamba ndi Padziko Lapansi ” Zaka 1,900 Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse isanayambe , Satana analonjeza Yesu kuti adzamupatsa “ maufumu onse a padziko . ” ( b ) Kodi lonjezo la Yehova limene lili pa Salimo 32 : 8 linakwanilitsidwa bwanji kwa inu ? Kodi mungafunse kuti n’cifukwa ciani Mulungu walola zimenezo kucitika ? ( b ) Kodi “ kukoma mtima kwakukulu ” kochulidwa pa Aroma 3 : 24 n’ciani ? ( Onani bokosi lakuti , “ Mautumiki Anthawi Zonse . ” ) Mtumwi Mateyu anagwila mau a Yesaya ponena za Yesu kuti : “ Bango lophwanyika sadzalithyola , ndipo cingwe ca nyale comwe catsala pang’ono kuzima sadzacizimitsa . ” ( Yes . 42 : 3 ; Mat . Mwanjila imeneyi , iwo amasiyana ndi atsogoleli ambili azipembedzo amakono ndi a m’zaka 100 zoyambilila . Timakhala na mtendele weni - weni ngati tidzimva kuti ndise otetezeka komanso ngati palibe cimene cikutivutitsa maganizo . Kodi Yesu anagwilitsila nchito bwanji luso lozindikila pamene anthu a ku Galileya anapita kukamufunafuna ? Ngakhale kuti Mulungu ali ndi maina ambili audindo , iye ali ndi dzina limodzi limene anadzipatsa yekha . — Ekisodo 3 : 15 . Ngakhale kuti anayesetsabe kucita zinthu zokondweletsa Mulungu , zioneka kuti sanaphunzilepo kanthu pa zimene iye ndi Ahabu anakumana nazo , komanso pa mau ocenjeza amene Yehu anamuuza . Tonse , acicepele ndi acikulile , abale ndi alongo , ‘ tingalimbikitse ’ Akristu anzathu amene afunikila thandizo . — Akolose 4 : 11 . 10 , 11 . ( a ) Kunyada kumaonekela bwanji ? Kuyendanso panyanja sikunali koopsa cifukwa asilikali aciroma anali kuteteza nyanjazo kwa anthu acifwamba . N’nali nisanaŵelengepo Baibulo , ndipo n’nakondwela kuphunzila za dzina la Mulungu na colinga cake . ( Mexico ) , Aug . Ngati munacitapo zinthu muli wokwiya , ndiye kuti yankho lake mwalidziŵa kale . Tingadziyese mwa kudzifunsa kuti : ‘ Kodi nimakhulupililadi kuti nili m’gulu limene Yehova akuseŵenzetsa pokwanilitsa cifunilo cake ? Conco , pamene ndinali ndi zaka zisanu , io anauza amai kuti akandilembetse pa sukulu ina yophunzitsa kuvina kudela lathu . 1 : 13 ) Ngakhale zinali conco , Yesu monga “ mbeu ” yolonjezedwa , anafunika kuyembekezela kuti apatsidwe mphamvu zolamulila dziko lapansi . Kodi Yehova amawaona bwanji atumiki ake padziko lapansi ? 4 , 5 . ( a ) Ndani angakupatseni thandizo lofunikila nthawi zonse ? William anati : “ Cimwemwe cimene tili naco cifukwa cogwila nao nchitoyi ndiponso kutumikila pamodzi ndi banja la Beteli sitingaciyelekezele ndi cinthu ciliconse . Kodi Akristu acikulile angathandize bwanji ena ndi cidziŵitso cao ? Phunzilani Kukhala Wodziletsa , Sept . Zotsatilapo n’zakuti anthu a Mulungu adalitsidwa mwa kukhala ndi akulu ndi atumiki othandiza ambilimbili . Muzicita maulaliki osiyanasiyana . 4 : 4 ) Njila imodzi imene Satana amasoceletsela anthu ambili ndi kuwacititsa kukhulupilila kuti iye kulibe . Iye anaphunzilapo Baibulo mobwelezabweleza ndi abale osiyanasiyana ndipo buku lake lakuti Chidziŵitso Chotsogolera ku Moyo Wosatha la zilembo za anthu akhungu linali litaonongeka . Tikamaganizila kwambili mmene amatikondela , cikondi cathu pa iye cimakula kwambili ndipo timafunitsitsa kutengela citsanzo cake . ( Miyambo 17 : 3 ) M’malomwake , Yehova anaona kuti Saulo angaumbidwe ndi kukhala ‘ ciwiya cocita kusankhidwa ’ kuti akalalikile “ kwa anthu a mitundu ina , komanso kwa mafumu ndi ana a Isiraeli . ” Tidzaphunzila kuti kunyadila nchito yocitila umboni za Yehova ndi Yesu kumafuna kuti tikhale acangu mu ulaliki . Kumafunanso kuti tizilemekeza Mulungu ndi Kristu ndi khalidwe lathu bwino . ( Gen . 39 : 11 - 15 ) Ngati tiganizila zotulukapo zoipa za chimo , tidzayamba kudana kwambili na coipa . Ganizilani za Sylviana , amene tam’chula kuciyambi kwa nkhani ino . Kodi ena a makhalidwe amenewo ndi ati ? Abale na alongo ocokela kosiyana - siyana amenewa , amatumikila Yehova mogwilizana . Koma Baibulo limanena za mkate wapadela kwambili umene sitiyenela kunyalanyaza . Kodi tingadziŵe bwanji nthawi yabwino yokambitsilana ndi anthu m’gawo lathu ? 4 , 5 . ( a ) Kodi kuleza mtima kumaphatikizapo ciani ? Malinga n’zimene Baibo imakamba , kuleza mtima ni mbali ya cipatso ca mzimu woyela . Conco , popanda thandizo la Mulungu , ise anthu opanda ungwilo sitingakwanitse kukhala oleza mtima pa mlingo wokwanila . N’ciani cimene Mulungu amapatsa anthu onse ? Palibe cinthu cofunika kwambili kuposa kutumikila Mulungu Wamphamvuyonse . Iye anati : “ Inu mukudziŵa bwino ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse , kuti pamawu onse abwino amene Yehova Mulungu wanu ananena kwa inu , palibe ngakhale amodzi omwe sanakwanilitsidwe . Inu Ayuda ndi anthu a ku Yerusalemu , musaope kapena kucita mantha . ” Tingapewe bwanji mzimu wokonda cuma ? Anthu a Yehova m’nthawi ya mapeto ino , ali ndi udindo wolalikila “ uthenga wabwino . . . wa Ufumu . . . padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse . ” N’tafika pafupi - fupi zaka 9 , atate , amene anali kudana na cinyengo ca m’machechi , anapeza mabuku ovumbula cipembedzo conama . Ataimba nyimbo ya Ufumu kwa nthawi yoyamba m’cinenelo cake , anati : “ Mukauze Bungwe Lolamulila kuti nyimbozi zikumveka bwino kwambili m’Cituvalu kuposa m’Cingelezi . ” Paulo anafotokoza bwino za vutoli . Kodi tingacite ciani kuti tikulitse mgwilizano wathu ? ( Yesaya 41 : 10 ) Conco , kuopa Mulungu kumatanthauza kukhala ndi mantha aulemu ndi kumulemekeza kwambili . ( b ) Ndi funso liti limene aliyense ayenela kudzifunsa ? 14 : 9 ) Mofananamo , anthu ambili anamva zimene Yesu anali kunena . Cifukwa ca zimenezi , iye waonetsa kuti ndi Mfumu yabwino kwambili ya Ufumu wa Mulungu . — Afilipi 2 : 8 - 11 . Ndipo amafuna kuti otsatila ake onse azicita cimodzimodzi . Anali kutilimbikitsa ndi kutithandiza panthawi imene zinthu zinali zovuta kwambili . ” Mwamunayo anakondwela kwambili ataona kuti mkazi wake wakhala wokhulupilika , ndi kuti wamvela cikumbumtima cake . Komabe , zosankha zambili zimene timapanga zingakhudze kwambili umoyo wathu . 24 : 44 ) Kupitila m’Baibulo , Mulungu na Khiristu watiuza madalitso amene atisungila kutsogolo , na zimene tingacite kuti tikhalabe maso . Ni zinthu ziti zimene zinasinthiwa m’buku la nyimbo latsopano ? A Inoki : Mfundo za m’Baibulo zingatithandize kudziŵa mmene tiyenela kuonela ndalama , kapena mmene tingakhalile ndi banja lacimwemwe , ndiponso mmene tiyenela kukhalila ndi anzathu . ( Aroma 7 : 24 ) Mau amenewa anakamba ni mtumwi Paulo . Umbombo umayamba pang’onopang’ono , koma ngati siticitapo kanthu , ungakule ndi kuononga moyo wathu . Ni malemba ati a m’Baibo amene anam’thandiza ? ( Dan . 2 : 30 ) Ndipo Danieli anali akali wacinyamata pamene Yehova anamuchula monga munthu wolungama pamodzi ndi Nowa , na Yobu . Tikakhulupilila nsembe ya dipo la Khiristu , ndiye kuti tasankha kuti tizilamulidwa ndi kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova . 15 : 39 , 50 ) Lingatanthauzenso cibale , kapena kuti cibululu . Mwacitsanzo , Yesu “ anatuluka m’mbeu ya Davide monga munthu [ “ mwa thupi , ” Buku Lopatulika ] . ” Yohane analinso na mwayi wapadela wobatiza Yesu , Mwana wa Mulungu wangwilo . “ Nditayamba kuphunzila Baibulo , ndinaleka cizoloŵezi canga cakumwa mankhwala osokoneza ubongo , kuledzela , ndipo ndaphunzila kuugwila mtima . Chivumbulutso 6 : 1 , 2 Dzikoli ladzala ndi ziphunzitso ndi zikhulupililo zacipembedzo zosokoneza . Ngati mtima wathu utilimbikitsa kucita zinthu mosonkhezeledwa ndi kunyada kapena umbombo , n’kwanzelu kuganizila zotsatilapo zake . Mukaona kuti m’bale kapena mlongo akudandaula za abale amene akutsogolela , musafulumile kusiya kukambitsana naye . Ngakhale kuti mamembala a cipani cao anali kugwilizana kwambili , makhalidwe monga kukondela , kufuna kuchuka , mikangano , ndi nsanje zinali zofala . ( Genesis 37 : 2 ) Mwinamwake kulimba mtima kumeneko kunacititsa Yakobo kukhala ndi maganizo oyenela kulinga kwa mwana wake wokondedwa . Ndithudi , Mulungu anadalitsa mlongoyo kaamba ka khama lake . Azibusa a Cikatolika anali kuletsa olamulila kuti asatipatse cilolezo cocita misonkhano yathu . ( Ŵelengani Miyambo 20 : 29 . ) YEHOVA afuna kuti tikhale acimwemwe , ndipo amatipatsa madalitso ambili kuti tikhale osangalala . Kodi zikuoneka kuti ndi liti pamene Petulo anasamukila kumalo osoŵa ? Baibo imathandiza ngakhale pa nkhani za umwini . Kumeneko , iye sanali kukhala ngati ali ku jele . Poonetsa kuyamikila zimene Alexandra anam’citila , mnyamatayo anamuitanila ku cakudya ku lesitilandi yake pamodzi ndi anzake amene anabwela nawo ku msonkhano . Ndinali kupita ku chechi nthawi zonse , ndipo ndinali kufuna kudzakhala mmishonale wa Katolika monga msuweni wanga amene anali ku Africa . Cifukwa cosamvela Yehova , Adamu na Hava anakanidwa na Mulungu monga opanduka . Mofanana ni wamasalimo , n’natulila Yehova nkhawa zanga ndipo iye ananicilikiza . Tikamapezeka pamisonkhano , timathandiza kuti mpingo ukhale wogwilizana . Iye anali na makhalidwe ambili abwino . Ndipo anthu mamiliyoni ambili a “ nkhosa zina ” amawacilikiza mokhulupilika . ( Lev . 15 : 25 - 27 ) Koma Yesu , amene anali kuzindikila kuti “ zinthu zofunika za m’Cilamulo , ” zinali kuphatikizapo “ cifundo ndi kukhulupilika , ” sanadzudzule mkaziyo cifukwa cogwila malaya ake . ( Mat . Ifenso tingapemphe Yehova kuti atithandize monga mmene anathandizila Davide . — Salimo 103 : 3 . Citsanzo cina ni Davide . Iye anafotokoza kuti kukhala paubwenzi ndi Atate wathu wakumwamba ndi kumene kumabweletsa cimwemwe . Conco , m’pomveka kuti kukhululuka ni cizindikilo cakuti munthu ali na cikondi , cimene “ cimagwilizanitsa anthu mwamphamvu kwambili kuposa cinthu cina ciliconse . ” 3 : 6 - 13 . United States 1,190,000 Pamene Jacqueline anali ndi zaka 16 , anaphunzila za sayansi yokhudza zinthu zamoyo ku sukulu . Abale ambili anakondwela atamva kuti sukuluyi idzayamba kucitika m’nthambi zambili . Kuyambila nthawi ya Adamu ndi Hava , Mdyelekezi wakhala akukopa anthu kuti akhale kumbali ya ulamulilo wake polimbana ndi Mulungu . Mtundu wa zilembo zake zokongola unapangitsa ena kukamba kuti “ zonse zionetsa kuti ni buku yocititsa cidwi . ” Anthu ambili masiku ano ayamba kulambila Yehova . Yehova anakamba kuti adzawawononga kothelatu . 10 : 1 , 2 ) Pambuyo pa zaka pafupifupi 150 , Yeremiya anapeleka uthenga wa Yehova kwa anthu a Mulungu osakhulupilika . Iye anati : “ Ine ndinakubzala ngati mtengo wa mpesa wofiila , wabwino kwambili . Mtengo wonsewo unali mbeu yeniyeni yabwino . Tingadzifunse kuti : ‘ Kodi nimaonetsa kuti ndine munthu amene sasungila ena zifukwa ? ( a ) Timadziŵa bwanji kuti Mulungu ndi Kristu amakonda anthu ? Koma pali mapempho ena anai amene atsala opezeka m’pemphelo lacitsanzo la Yesu . Woweluza Gidiyoni anatumikila Yehova panthawi yovuta pambuyo pakuti Aisiraeli alowa m’Dziko Lolonjezedwa . Kodi anthu amene ‘ amachula dzina la Yehova aleka kucita zosalungama ’ m’njila zina ziti ? N’cifukwa ciani n’kovuta masiku ano kuika maganizo athu pa zinthu zofunika kwambili ? Tidzakambilana funso liti ? Kodi ni liti pamene amuna amenewa anakwela pa mahosi na kuyamba kuthamanga ? Iko kanamwetulila ndi kuyankha kuti , “ Inde , nidziŵa . ” Ndiponso , panali anthu 750 sauzande amene anaticezela kuphatikizapo Mfumukazi Elizabeth wa ku England . ( Tito 1 : 2 ) Popeza analonjeza zinthu zonse izi zabwino m’tsogolo , cingakhale canzelu ise kudzifunsa kuti : Kodi n’zoona kuti anthu adzakhala kwamuyaya m’Paradaiso wolonjezedwa padziko lapansi ? Ndipo nthawi yomweyo mtsikanayo anauka . Koma bwanji ngati mumalephela kukamba ndi anthu a m’gawo lanu za Yehova ndi Ufumu wake ? Iwo anangolemba uthenga umene Mulungu anawauza . Iwo anayamba kucitila umboni za Ambuye , ndi kutsimikizila kuti Yehova ali na mphamvu zoukitsa akufa . — Mac . Cikondi ndi khalidwe limodzi mwa makhalidwe abwino ambili a Mulungu , ndipo ndi khalidwe lake lalikulu . Iye ndi gulu lake afuna kuti aja amene akukalamila azimutumikila mokondwela . Inetu ndangofunsa cabe . ” Malemba amamucha “ wolamulila wa dzikoli ” ndi “ mulungu wa nthawi ino . ” ( Yoh . 12 : 31 ; 2 Akor . Kodi tingapatule nthawi pambuyo pa misonkhano kuti tithandize munthu wina amene akufunikila thandizo ? Pocita misonkhano yampingo ndi ikulu - ikulu , m’gulu mumakhala anthu osiyana - siyana monga acatsopano , okondwelela , acicepele , na alongo . Anthu amenewa akamaimba nyimboyi , zinali kukhala ngati kuti akuuza ena zofunika kucita . 24 : 7 , 11 , 12 , 14 ; Luka 21 : 11 ) Apa tingoyembekezela mwacidwi mmene kubwela kwa Yesu kudzatipindulitsila ndi kukwanilitsika kwa cifunilo ca Mulungu . — Maliko 13 : 26 , 27 . Baibo imalonjeza kuti : “ Ukaitana kumvetsa zinthu . . . , udzamudziŵadi Mulungu . ” — Miyambo 2 : 3 - 5 . ( 1 Yohane 2 : 17 ) Popeza mapeto a dzikoli ali pafupi , ino ndiyo nthawi ‘ yoyembekezela Yehova , ndi kusunga njila zake . ’ — Salimo 37 : 34 . Paulo analemba kuti : “ Anthu onse adziŵe kuti ndinu ololela [ kapena kuti oganiza bwino ] . ” Panthawiyo , m’dziko lawo la Bosnia munali nkhondo ya pakati pa mitundu yosiyana - siyana . Nditumizeni . ” — Yes . Tikasankha Yehova kukhala Mulungu wathu ndi kumukhulupilila monga mmene Davide anacitila , tidzakhala olimba mtima tikakumana ndi mavuto . 45 : 1 - 5 ) Yehova anakamba kuti adzawononga mzindawo ndipo sadzateteza katundu wa munthu aliyense . Limeneli ndilo lamulo lalikulu kwambili komanso loyamba . ” — Mat . Jowana anatumikila Yesu ndipo anali wokhulupilika kwa iye ngakhale pamavuto . Conco , ngakhale tione kuti tayembekezela nthawi yaitali , zimenezo sizitanthauza kuti mapeto ali kutali kapena kuti sadzabwela ife tili moyo . 8 : 30 ) Pamene Yehova ndi Yesu anali kugwila nchito limodzi , Yesu anaphunzila zambili ponena za makhalidwe a Atate wake . Zimenezi zinaŵacititsa mantha cifukwa anaganiza kuti ndine mmodzi wa akuluakulu a boma . Gwen : Kudzipeleka pa nchito yathu yovina kunali kosangalatsa , koma cisangalalo cake cinali ca kanthawi . NYIMBO : 112 , 133 Mkati mwa “ nyengo yabwino koposa ” imeneyi , panali kucitika makampeni apadela , omwe anali kupatsa anthu mwai woonetsa ciyamikilo cao kaamba ka dipo . Nthawi zina , zimavuta kudziŵa ngati munthu ni wolapadi kapena ayi . Titayamba kuphunzila Baibulo ku Germany , ine ndi Laurie tinasamukila ku France , patapita nthawi tinasamukila ku Italy . Tinapemphelanso kuti Yehova atithandize . Koma kuŵelenga Baibo kwanithandiza kukhala na umoyo watanthauzo . N’cifukwa ciani tifunika kucita khama kuti timvetsetse na kutsatila mfundo za m’Baibo pankhani yolemekeza ena ? Tinali kuima pa mzele wogula zakudya kwa maola ambili koma cakudya cinali kutha tisanagule . Panthawi yake , Yehova adzavumbula onse amene amacita zoipa kapena a moyo wapaŵili , ndipo adzasiyanitsa “ pakati pa munthu wolungama ndi woipa ndiponso pakati pa munthu amene akutumikila Mulungu ndi amene sanatumikilepo Mulungu . ” Mayankho ocepa amene anandipatsa anali acabecabe ndipo sanandifike pamtima . Iwo anali kukhalila kundiyang’ana . Conco , kwa milungu yambili ndinali kukhala m’nyumba . Koma Yesu sanali kuona atumwi ake monga akapolo . ( Yohane 5 : 28 , 29 ) N’naphunzilanso kuti Mulungu amanikonda . Coyamba , tinali kupita kukaonana ndi anthu apamwamba monga meya wa mzinda . Ndiyeno , tinali kupita kunyumba ndi nyumba kukagaŵila mabuku athu . Mkulu wina amene anatsitsidwapo anati : “ Tsopano ndadziŵa mocitila ndi aja amene amalakwa . ” Ndiyeno , anayamba kugwila nchito imene siinali kukhudzana ndi zausilikali . Kodi sadzacitapo kanthu ? ’ — Sal . Aliyense amene ali pakati panu mwa anthu onse amene amamutumikila , Yehova Mulungu wake akhale naye . Kunena zoona , cikondi , cifundo ndi kukhululukila ndi makhalidwe ofunika kwambili . ( Miy . 31 : 10 , 27 , 28 ) Ngati ana amamvela makolo ao akulankhula za Yehova ndi kuŵaona akum’tumikila tsiku lililonse , naonso angayambe kucita zimenezo . ZOTSATILAPO ZOSAYEMBEKEZELEKA Ndiyeno m’pempheni kuti achule thandizo limene angapeleke kwa anzake . Akatswili ofufuza zinthu amakaikila ngati gulaye inali m’gulu la uta . Utsi umene munthu amatulutsa akamakoka , ndi umene umatuluka poumitsa fodya ndi wovulaza . Tinadziŵa kuti anali kunama , ” anatelo a STEPHEN . ( b ) Koma kodi “ kuika maganizo pa zinthu za mzimu ” sikutanthauza ciani ? Mwacitsanzo , mungamvele bwanji ngati inu kapena mnzanu wacotsedwa pa udindo kapena pa utumiki umene anali kuukonda ? Ngakhale n’conco , nthawi yakuti Mulungu abweletse mtendele weni - weni sinakwane . Kucita conco kudzaonetsa kuti amaona cilango ca Yehova kukhala umboni wa cikondi cake . “ [ Lamulo ] laciŵili lofanana nalo ndi ili : ‘ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ’ ” — MATT . Ndipo tonse tiyenela kucitapo kanthu kuti mpingo ukhalebe wogwilizana . Kwa zaka zambili , mabuku athu afotokoza kuti zimene Yesu anakamba ponena za cikwati pambuyo pa ciukililo , zimatanthauza ciukililo ca padziko lapansi . Ndipo kuti aja amene adzaukitsidwa kukhala ndi moyo m’dziko latsopano sadzakwatila kapena kukwatiwa . * ( Mat . Kuti tikhalebe odzicepetsa , nthawi zonse tifunika kupatula nthawi yosinkha - sinkha zimene timaŵelenga m’Baibo . 94 : 20 ; Chiv . Komanso , akulu mumpingo amapanga makonzedwe oyendela ndi kuthandiza anthu ocotsedwa a m’gawo la mpingo wawo , amene aoneka kuti analeka kucita macimo . N’cifukwa ciani Yesu anagwilitsila nchito mau akuti “ zolakwa ” kapena kuti nkhongole koma pambuyo pake anakamba za “ macimo ” ? ( Mat . Paulo anauza anthu a ku Lusitara amene anali kupembedza mafano kuti : “ Mulungu wamoyo . . . sanangokhala wopanda umboni wakuti anacita zabwino . Anakupatsani mvula kucokela kumwamba ndi nyengo zimene zokolola zanu zimakhala zambili . Kodi anthu ena anakuvutitsamponi cifukwa cocita zinthu zabwino molimba mtima ? Ngakhale masiku ano , aliyense wocita zimenezi ‘ amanyoza mzimu wa Mulungu , yemwe amasonyeza kukoma mtima kwakukulu . ’ — Aheb . Kutalika kwa nthawi imene anthu ofedwa amakhala na cisoni kumasiyana - siyana . Yehova anadalitsa Rute mwa kum’patsa mwamuna ndi mwana . Olo kuti n’nali wam’ng’ono , n’nali kudziŵana ndi akulu - akulu andale ochuka a m’dziko la GDR . Maboma angapeleke cakudya , zovala , ndi malo okhala , koma cakudya cimene angawapatse cingakhale cosiyana kwambili na cimene anajaila . Kapena nimayesetsa kupeza mipata yothandiza abale na alongo amene siniwadziŵa bwino kapena amene ni osoŵa ? ’ Tikamaganizila mfundo za m’Baibo , cikumbumtima cathu cimatitsogolela bwino ( Onani palagilafu 16 ) Buku yakuti Encyclopædia Britannica imafotokoza kuti umbeta ni “ kukhala wosakwatila kapena wosakwatiwa komanso kupewa kugonana , nthawi zambili cifukwa ca udindo umene m’busa wacipembedzo ali nao , kapena pa cifukwa cakuti munthu ni wokangalika pa zacipembedzo . ” Nkhani yotsatila idzafotokoza Malemba ena amene amakamba zimene anthu anaona m’masomphenya . N’nayamba kukonda kwambili zimene n’nali kuphunzila . Mdani wamkulu amene tikulimbana naye ni Satana ndi dziko lake loipa . ( Aef . Kodi Yesu anawalimbikitsa bwanji atumwi ake , maka - maka Petulo ? ( Luka 1 : 46 - 55 ) Zoonadi , Yehova anali kuona zimene Mariya anali kucita , ndipo cifukwa ca kukhulupilika kwake anam’patsa mwayi wapadela umene sanali kuuyembekezela . Tiyenela kuona munthu amene wasiya mpingo monga “ nkhosa yosocela ” osati ngati munthu woipa woti sangabwelelenso m’gulu la Yehova . Tate wacikondi amateteza banja lake ku ngozi . Nanga n’ciani cimapangitsa kuti munthu acotsedwe ? Mu 1553 , Iye anafalitsa Baibulo loyamba lathunthu m’cinenelo ca Cifulenci lokhala ndi macaputala ndi mavesi amene ali m’Mabaibulo ambili masiku ano . Ngakhale kuti mwina “ Seŵelo la Eureka ” silikumbukika kwambili , anthu mamiliyoni analipenyelela kuyambila ku Australia mpaka ku Argentina , ku South Africa mpaka ku zilumba za ku Britain , ku India , ndi ku Caribbean . ( Mat . 20 : 28 ) Monga munthu wangwilo , Yesu anali kudzapeleka “ dipo . ” NKHANI YA PACIKUTO | KODI MAPETO A DZIKOLI ALI PAFUPI ? Kodi anali osiyana bwanji ? Onani Buku Lapacaka la Cizungu la mu 1988 pa mape . Mlongo wina wa ku Japan , wochedwa Michiko , anakakamizidwa ndi acibale ake kukwatiwa ndi munthu wosakhulupilila . Koma tsopano muli ofalitsa opitilila 200,000 , kuphatikizapo atumiki a pa Beteli ambili amene akucilikiza nchito yofunika kwambili yolalikila . Yesu asanapeleke pemphelo lacitsanzo limeneli anati : “ Popemphela , usanene zinthu mobwelezabweleza . ” ( Mat . Koma limatithandiza kuyandikila kwa Mulungu . Koma sitiyenela kumangopempha zinthu zakuthupi . Mulungu anapanga munda wokongola kuti anthu akhalemo , ndipo anawalenga ndi maganizo ndi matupi angwilo kuti akhalepo kwamuyaya . 1 : 28 ; 9 : 1 ) Baibo siikamba kuti Akhristu nawonso ayenela kutsatila lamulo limeneli . Ndinali kukwiya msanga ndiponso waciwawa . Kunyada ndi umbombo zimatsogolela ku ngozi . Malinga n’zimene acicepelewa anafotokoza , pamene mwakonzekela bwino ulaliki m’pamenenso “ nsapato ” zanu zophiphilitsa zimakhala zogwila bwino ku mapazi anu . Ali kumeneko , iye na mnzake Sila anamangiwa pa mlandu wabodza , ndipo anaponyedwa m’ndende . Amuna ndi akazi okhulupilika amenewa anali kupemphela kwa Mulungu yekha . — Afilipi 4 : 6 . Kaya anawo akhale ndi luso lotani , makolo ao amakondwela kudziŵa maluso ao . Mukakumana ndi mavuto paumoyo wanu , kodi mumada nkhawa kwambili ? Kuti tikalandile mphoto , tifunika kukhala na cikhulupililo conse mwa Yehova ndi kulabadila malangizo ake . Mwamsanga , Nowa anamanga guwa lansembe ndi kupeleka nsembe kwa Yehova . * — Miyambo 18 : 1 . Yehova anatilenga m’njila yakuti tizisangalala , n’cifukwa cake akutilonjeza kuti ‘ adzakhutilitsa zokhumba za camoyo ciliconse . ’ ( Sal . Conco , tiyenela kupewa kudziona monga tili na udindo wopangila abale ndi alongo zosankha . M’malo modzisankhila zimene tifuna kusintha , tifunika kulola Mulungu kutitsogolela . ( Eks . 34 : 6 ) Mulungu amalemekeza atumiki ake . Zinthu zikatelo , cikhulupililo cathu mwa Yehova cingafooke . “ Kale simunali mtundu , koma tsopano ndinu mtundu wa anthu a Mulungu . ” — 1 PET . Onani nkhani 9 m’buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . 2 : 6 - 8 ) Ambili anali amuna a maudindo mumpingo . Anali kutumikila monga oyang’anila , koma m’kupita kwanthawi , anakhala “ mabishopu . ” 9 , 10 . ( a ) Panthawi yocepa ya bata , kodi anthu a Mulungu adzalengeza uthenga wotani ? Koma iye anali kudela nkhawa kwambili anthu . Akamayenda , Rabeka anali kufunsa mafunso Eliezere , kuti adziŵe zambili zokhudza Isaki ndi banja lake . Nthawi zina tingaone kuti kucotsa munthu mumpingo ndi nkhanza , makamaka ngati munthuyo ndi m’bale wathu . ( Mateyu 24 : 3 , 7 ; Luka 21 : 10 , 11 ) Nkhondo yoyamba ya dziko lonse itayamba mu 1914 , umboni unaonekelatu wakuti mtundu wa anthu waloŵa m’nthawi yovuta imene Baibo imakamba kuti “ masiku otsiliza . ” — 2 Timoteyo 3 : 1 - 5 . Wosalemekeza Mwana salemekeza Atate amene anamutuma . ” — Ŵelengani Salimo 2 : 11 , 12 . Panthawiyo , iwo anacita kukwela kumtenje kuti apulumuke cigumulaco . Koma ngati muona kuti sindinu okonzeka , gwilitsilani nchito malangizo amene ali m’nkhani ino kuti mupite patsogolo . Njila imodzi imene tingaonetsele kuti ndife okhulupilika kwa Yehova ndi mwa kulemekeza mwamuna kapena mkazi wathu , ngakhale kuti satumikila Yehova ( Onani ndime 9 ) Kodi Yesu anawalimbikitsa bwanji anthu ena ? Posankha zosangalatsa , kodi nimaganizila mmene Yehova adzaonela zosankhazo ? ’ Ngati timaphunzila Mau a Mulungu , kuwasinkhasinkha , ndi kugwilitsila nchito zimene timaphunzila , tidzaphunzitsa bwino cikumbumtima cathu . Ndiyeno anati : ‘ Koma inu osayang’ana umphawiwo . 12 Coonadi ‘ Sicibweletsa Mtendele Koma Lupanga ’ 3 : 1 - 3 . Yesu asanaukitse mtsikanayu , ananenanso kuti mwanayo anali m’tulo . — Luka 8 : 52 . Inu mudzaitana ndipo ine ndidzayankha . Anagwilitsila nchito Baibulo ponditsimikizila kuti Yehova amandikonda , ndipo anapemphela nane . Cishango cimeneci cinali kumuteteza ku zida zina na mivi imene adani anali kuponya . Yesu anakamba kuti limeneli ndilo lamulo lofunika kwambili . Kodi amene ali m’cikwati na mnzawo wosakhulupilila afunika kukhala na kaonedwe kotani ? Muzisunga nkhani zopezeka m’zofalitsa zathu kapena Malemba amene angakuthandizeni kulimbana ndi zofooka zanu ndipo muziwaŵelenga nthawi ndi nthawi ( Onani ndime 15 ) Conco , iye anapempha Sauli kuti apite naye padenga la nyumba yake . Tambani vidiyo yakuti , N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo ? Lemba la Salimo 146 : 3 limati : “ Musamakhulupilile anthu olemekezeka , kapena mwana wa munthu wina aliyense wocokela kufumbi amene alibe cipulumutso . ” Timafunikanso kuvala umunthu watsopano . Kumeneko io adzaika m’manda Gogi pamodzi ndi khamu lake lonse . ” Vikwati ivi vinali vosemphana ndi cilengedwe . Koma kodi muona kuti masiku ano zimakuvutani kusintha zinthu zing’onozing’ono kuti mutengele citsanzo ca Yehova ndi Yesu ? Ndi nchito zotani zimene Yehova anapatsa Adamu ? Olo kuti tikukhala “ pakati pa m’badwo wopotoka maganizo ndi wokhotakhota , ” timafuna kuti anthu aone kuti ndise ‘ opanda cifukwa cotineneza naco ndiponso osalakwa , ’ owala ‘ pakati pawo monga zounikila m’dzikoli . ’ ( Afil . Mwacitsanzo , ngati inu munali ndi Mose ndipo munamva pamene Aroni anali kufotokoza cifukwa cimene anapangila mwana wa ng’ombe wa golide , kodi mukanamuganizila ciani Aroni ? Kudziŵa kuti zinthu zoipa zimacitika , kumacititsa munthu ‘ wocenjela amene waona tsoka kubisala . ’ Mboni za Yehova zinali kugwilitsila nchito wailesi imeneyi kuyambila mu 1924 mpaka mu 1957 . Kodi machalichi acikristu amalalikila uthenga wabwino mmene Yesu anacitila ? Ndithudi , Yehova amayamikila kwambili zonse zimene atumiki ake amacita kuti akhalebe okhulupilika . — Ŵelengani Aheberi 6 : 10 , 11 . M’malo moopa zimene zicitike mtsogolo , mungayembekezele mapetowo mokondwela . Kodi Baibulo limatithandiza bwanji kupewa kunyada ndi kusankhana mitundu ? 3 : 10 ) Odzozedwa okhulupilika adzalamulila ndi Kristu kwamuyaya monga mafumu kumwamba , cifukwa cakuti ali m’pangano la Ufumu . Kodi inuyo mwatsimikiza mtima kucita ciani cokhudza malo athu olambilila ? Magaziniwo anali kuphunzitsa kwambili kuti dipo ndi njila yaikulu imene Mulungu anatisonyezela cikondi . Magazini ya Watch Tower inacha cikumbutso ca imfa ya Kristu kuti “ nyengo yabwino koposa . ” Musamaone kuti nsembe ya dipo la Yesu imapindulitsa cabe anthu monga gulu . Tonse tifunikila kuyesetsa kusakwiya msanga , na kukhululukila ena . Koma nthawi zambili , amatipatsa mphamvu kuti tithe “ kupilila zinthu zonse ndi kukhala oleza mtima ndiponso acimwemwe . ” Pa Danieli 12 : 8 , iye anakamba kuti : “ Tsopano ine ndinamva zimene ananenazo , koma sindinadziŵe tanthauzo lake . ” 12 : 35 , 36 ) Farao anacititsidwa manyazi ndipo anaphedwa . A Yohane : Ndikuona kuti sizingakhale zovuta . Tiyeni tiganizile citsanzo ca Danieli . Koma kunena zoona , nditangophunzila coonadi sindinali kucita zinthu mosamala , makamaka polalikila acibale anga . “ Khulupilila Yehova Ndipo Cita Zabwino , ” Jan . Tikamaphunzila za Yehova ndi malonjezo ake , timayamba kum’konda ndipo timayamikila zonse zimene waticitila . Pamene mucita izi dzifunseni kuti , ‘ Ndaphunzila ciani m’Mau a Mulungu ndi gulu lake ? ’ N’cifukwa ciani ciyamikilo cathu ciyenela kukhala cocokela pansi pa mtima ? Ndipo dziŵani kuti njila zolalikilila m’cimodzi - modzi padziko lonse . Pa 07 : 00hrs tsiku lokonkhapo , mukawapeza afika kale pa malowa . 9 : 22 ) Tonse atatu — Ine , Paul Bruun , na Raymond Leach — anatitumiza ku Philippines . Posacedwapa , Ufumu umenewu udzathetsa maboma onse a anthu . — Ŵelengani Salimo 2 : 2 , 7 - 9 . Munali mu 1941 pamene atate anaopseza amayi na mau amenewa . Koma comvetsa cisoni n’cakuti ena analephela kukhala ndi umoyo wosalila zambili . Iwo anavutika maganizo kwambili . Kwa zaka zambili , anthu a Mulungu anali kuona kuti kufotokoza nkhani za Baibulo mwa njila imeneyi kunali kolimbitsa cikhulupililo . Ngakhale kuti sunali kunikomela , n’nali kuukonda cifukwa n’nali kuledzela nawo . Ndipo kudzicepetsa kumeneku kunamuthandiza kucita zambili mu ulaliki . Ku Seoul , m’dziko la Korea , mu 1963 Yobu ? Angela Romano ni mmodzi wa alongo amene anali kubwela kudzaseŵenza nafe . ( 1 Petulo 3 : 7 ) Kodi inu amuna mungacite bwanji zimenezi ? Ndipo anaonjezela kuti : “ Conco pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse . ” ( Mat . Pa nthawiyo , m’tauni ya Mistelbach imene ananitumizako munalibe Mboni . Komabe , m’Malemba Aciheberi mulibe mau ogwilizana ndi amene Paulo anagwila . Conco , kukhala na pulogilamu ngati imeneyi , kungakuthandizeni kukulitsa cikondi na ciyamikilo canu pa Yehova na Yesu . Izi zidzakuthandizani kuti mukapindule mokwanila pa Cikumbutso . Atate anali kuletsa Amai kupita ku misonkhano . Nimaona kuti zaka 61 zimene nakhala nikutumikila pa Beteli zatha mofulumila kwambili . Kodi “ kubala zipatso ” kutanthauza ciani ? Onani kabuku kakuti , ‘ Onani Dziko Lokoma ’ mapeji 32 - 33 . Kuti mudziŵe zambili , onani Nsanja ya Olonda ya August 1 , 2008 , masamba 10 - 12 . Yehova na gulu lake ndiwo amatiitana ku phwando lauzimu limeneli . Ulamulilo wa anthu wacititsa nkhondo zambili zimene zapha anthu mamiliyoni . Pa tsamba lothela lililonse pali kamutu kakuti “ Ganizilani Funso Ili . ” 9 , 10 . ( a ) Kodi pali masukulu otani amene amatithandiza pa nchito yolalikila ? Komabe , ofalitsa ena sakhalanso ndi cimwemwe potumikila Mulungu . Iye akucita khama kuti ayenelele kusenza maudindo mumpingo . Funso limenelo linandigwila mtima . 13 : 20 . ( Onani palagilafu 13 - 15 ) Kucokela mu 1914 , anthu onse akudzionela okha “ cizindikilo ca kukhalapo kwa [ Kristu ] “ monga wolamulila wa dziko lapansi . ( Mat . Dziŵani kuti Yehova amakondwela mukamamvela Mau ake . ( Aroma 1 : 1 ) Anthu amene amalandila uthenga wa Ufumu wa Mulungu amawayanja kupyolela mwa Yesu Kristu . ZIMENE BANJA LIYENELA KUCITA Mwacionekele , na imwe mudziŵa kuti ngati makolo anu amakupatsani malangizo , ndiye kuti amakukondani . ( Aheb . Cida cina cimene cinali kugwilitsidwa nchito pambuyo pa caka ca 1930 ndi galamafoni yonyamulila m’manja . ( Luka 22 : 28 - 30 ) Kuti atumwiwo akalandile mphoto yawo , coyamba anayenela kufa . Pambuyo pake , tinapita kukafunafuna anthu ena a ciyela kuti tiwamenye . Nanga bwanji ngati mavuto a m’banja akutidetsa nkhawa ? Mlongo wina dzina lake Sylvie , amene watumikila pa Beteli ku France kwa zaka zambili , anakamba kuti alongo naonso angayamikile abale . Mwacitsanzo , onani nkhani yakuti “ Kodi N’zotheka Kucita Zinthu Mwacilungamo m’Dziko Laziphuphuli ? ” Malinga ndi fanizo la Yesu , ( a ) kodi mkwati ndani ? Mwacitsanzo , iye anafotokoza mmene Yehova amadyetsela mbalame pofuna kutsimikizila ophunzila ake kuti sayenela kuda nkhawa kuti adzadya ciani . Ndithudi , dziko lamtendele likubwela . Ndinaphunzila Kuti Yehova ndi Wacifundo ndi Wokhululukila 12 Ngati ali ndi ludzu , um’patse cakumwa . ” ( Aroma 12 : 20 ; Miy . Pofuna kufotokoza colingaco , Paulo anagwilitsila nchito citsanzo ca Aisiraeli amene anapulumutsidwa kwa Aiguputo . N’cifukwa ciani tifunika kukamba mokoma mtima ? ( Luka 19 : 43 , 44 ) Malipoti akuonetsa kuti anthu “ pakati pa 250,000 na 500,000 anafa mu mzinda wa Yerusalemu komanso mu Yudeya monse . ” Kuyambila kale - kale , anthu akhala akuidziŵa bwino mfundo imeneyi . ( Mat . 6 : 9 , 10 ) Kuti tikulitse ciyamikilo cathu kaamba ka dipo , tiyeni tikambilane mmene dipolo limagwilizanilana ndi kuyeletsedwa kwa dzina la Mulungu , ulamulilo wa Ufumu wa Mulungu , ndi kukwanilitsika kwa colinga ca Mulungu . Pamene mneneli Samueli anacedwa kufika ku Giligala , Sauli anataya mtima . N’zoona kuti umoyo wodalila thandizo la ena ungacotsele ulemu abale othaŵa kwawo , ndi kusokoneza ubale wawo ndi Akhristu ena . ( 2 Ates . Kukamba zoona , tonse mumpingo , kaya ndise acicepele , acikulile , kapena okondwelela , tingathe kulambila Yehova mwa kuimba nyimbo za Ufumu . Mwacitsanzo , nyimbo 12 zoyambilila zimakamba za Yehova , nyimbo 8 zokonkhapo zimakamba za Yesu na dipo , ndipo nyimbo zina zonse zinasanjidwa motsatila dongosolo limeneli . Mmodzi wa io anapeza lesitilanti kumene amaphika cakudya cocedwa falafel . Anthu m’dzikoli saganizila za moyo wao wa m’tsogolo . Conco , sitiyenela kukhala ndi cinthu ciliconse cimene cingatilepheletse kutengela citsanzo ca Yesu . — Mateyu 5 : 29 , 30 ; Afilipi 4 : 8 . Kuuka kwa Kristu kumatithandiza kuti tizilalikila molimba mtima . Mosataya nthawi , wacikulileyu amene kale anali mphunzitsi , anandiuza kuti safuna kuti tizifika pakhomo pake . Iwo ndi okondwa kuona kuti mukupilila ndi kukhalabe okhulupilika kwa Yehova . Tumapepala twa uthenga tumene tunatuluka mu 2013 , tunakonzedwa kuti tutithandize kucita zimenezi . Koma Yehova amafuna kuti tizilankhula naye momasuka . Mwa mau acidule ndi amphamvu otsatilawa , Baibo imatiuza zimene Yehova amafuna kucitila anthu omufuna - funa . Imati : “ Mitima yanu ikhale ndi moyo kosatha . ” — Salimo 22 : 26 . 6 : 11 ) Kodi Zekariya anauziwa kuti cisotico akaveke Bwanamkubwa Zerubabele , amene anali wa fuko la Yuda ndi mbadwa ya Davide ? Kodi kucitila anthu amene timalalikila zinthu zimene tingafune kuti io aticitile kuli ndi ubwino wotani ? ( 1 Mbiri 28 : 9 ) Mboni za Yehova zidzakhala zokondwela kukuthandizani kufunafuna Mulungu wosaonekayo ndi kum’peza . [ Mau okopa papeji 15 ] Onani “ Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga ” mu Nsanja ya Olonda ya December 15 , 2001 . Koma zimenezi sizinacitike . Pamene tinacoka ku Tuvalu , tinatumizidwa ku ofesi ya nthambi ya ku Samoa mu 1985 . Ngakhale mabungwe amene amati ni osungitsa mtendele , monga United Nations , alephela kuimitsa wokwela pa hosi yofiila . Nthawi zonse Akhristu anzanga anali kunithandiza . ” Mungacitenji kuti muthandize ana kuti asataike ? Ndiye cifukwa cake anapeleka mwana wake wokondedwa kuti ise tikhale na ciyembekezo ca moyo wosatha . — Ŵelengani Masalimo 84 : 11 ; Aroma 8 : 32 . Pamsonkhanowo , M’bale Knorr anakamba kuti anthu a Mulungu afunika Baibulo lomasulidwa mwamakono . Baibulo limenelo linafunika kukhala lolondola , losavuta kumva , limenenso lingathandize anthu kuphunzila coonadi mosavuta . Kuwonjezela apo , tapanga masinthidwe ofunikila kuti titumikile abale athu . Koma pambuyo pa zaka 25 , io anapita kukaceza kudela limenelo . Tsopano cotsani moyo wanga Yehova . ” Ndi mmenenso zidzakhalila m’dziko latsopano . Banjalo linali kulimbikitsa abalewo kutsatila malangizo amene linawapatsa , koma ena sanatsatile . Ngakhale kuti n’nali na mkazi , n’nalinso na akazi ena akumbali . Izi zingafooketse cikhulupililo cathu , ndipo ‘ tingakhale aulesi ’ potumikila Yehova . — Aheberi 6 : 10 - 12 . 4 : 4 ) Conco , iye anawalembela kalata . Nanga masiku ano timapindula bwanji ndi misonkhano ? Anthu sangathe kuzindikila kuti ndi nkhani ziti za m’Baibulo zimene zimaimila zinthu zodzacitika mtsogolo kapena ai . Yesu analimbikitsa ophunzila ake kuti ayenela kuonetsa kuwala kwawo kuti Mulungu alemekezeke . Ngakhale kuti bungwe lolamulila linali kutsogolela mpingo woyambilila , linali kudziŵa kuti Mtsogoleli wawo anali Yesu . “ Kwa ine , kulemekeza mwamuna wanga kumatanthauza kumuonetsa m’zocita zanga kuti nimam’konda , ndipo nimafuna kuti azikondwela . Ndinali kudziŵa ndithu kuti akufa , koma ndinayesetsa kuwalimbikitsa popanda kuonetsa nkhawa iliyonse . Kodi mau ouzilidwa amenewa akunenanso Mboni za Yehova za lelolino ? Izi zinacitika zaka zoposa 3,000 m’mbuyomu , ndipo kuonetsana cikondi mwa njila imeneyi kungaoneke kwacilendo kwa ife masiku ano . 104 : 14 , 15 ; Mlal . 3 : 12 , 13 ) N’ndani amene sakondwela ngati apuma mpweya wabwino , kudya cakudya cokoma , kapena kugona tulo twabwino ? Mzimu wa Yehova ungatithandize kupita patsogolo . Cimakula m’kupita kwa nthawi Anthu ena samvetsetsa mau ouzilidwa akuti : “ Ciliconse cili ndi nthawi yake , . . . pali nthawi yobadwa ndi nthawi ya kufa . ” Mtumwi Petulo anaonetsa mzimu wodzimana pophunzitsidwa ndi Yesu . N’cifukwa ciani tingakambe kuti tili na zonse zofunikila kuti tithe kupanga zosankha mwanzelu ? Ayuda okamba Cigiriki anadandaula kuti akazi amasiye awo anali kunyalanyazidwa . ( Mac . “ Zinthu zimenezi . . . zinalembedwa kuti ziticenjeze ifeyo amene mapeto a nthawi zino atifikila . ” — 1 AKOR . Conco , ngati muona kuti pakali zina zimene simucita bwino , musataye mtima . pophunzitsa pa pulatifomu ? Koma anadziŵa kuti ambili mwa anthuwo ndi Abuda ndipo sadziŵa kwenikweni zimene Baibulo limanena . Komabe , anthu m’mbali zina za dzikoli akuyesetsa kuthetsa nkhanza . Akhristu amaona moyo kukhala wofunika kwambili kuposa zinthu zakuthupi . Ofalitsa akapita ku maulendo obwelelako kwa anthu amene anasiila buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu , kaŵilikaŵili amapeza kuti eninyumba ayamba kuŵelenga bukulo kapena alimaliza . Komabe , monga bwenzi la Mulungu , sanalole mkwiyo kufooketsa cikhulupililo cake . Kuuka m’maŵa kuti tipite mu ulaliki nthawi zina kungafune kuti tidukize tulo . Nanga anthu amene atumikila ku Micronesia amapeza madalitso otani ? Amene amacita zimene angathe muutumiki amaonetsa kuti ali ndi cikhulupililo colimba ( Onani ndime 13 ) Cikondi cidzatithandizanso kuganizila zofuna za ena osati zathu zokha . — Afil . Ngati palibe , bwanji osasakila bwenzi la conco ? Zili conco cifukwa cakuti m’miyala ina mungapezeke cabe golide wolemela magalamu 10 . 6 : 10 ) Pemphelo limeneli lidzayankhidwa kothelatu pamene dziko loipali lidzacotsedwa . Cokondweletsa n’cakuti tinazindikila kuti kucita zinthu nthawi imeneyo pamene tili ndi mkwiyo sikuthandiza . Tikalibe kudziŵa Yehova , mwina tinali ndi makhalidwe ambili oipa . Iye anali na mwayi wokaphunzila za malamulo ku univesiti , koma m’malomwake anasankha kuyamba kugwila nchito ya malipilo ocepa . Pozindikila kuti kukhalapo kwa Kristu kunayamba mu 1914 , otsatila a Yesu anadziŵa kuti mapeto ali pafupi . KODI timadabwa kuti tiyenela kukumana ndi “ masautso ambili ” tisanalandile mphoto ya moyo wosatha ? N’zocititsa cidwi kuona zimene Yesu ananena pa Mateyu 5 : 38 , 39 . Iye anati : “ Inu munamva kuti , ‘ diso kulipila diso , ndi dzino kulipila dzino . ’ Koma kodi anaonetsa bwanji kukhulupilika ? Ndipo mwina Mose anayamba kuganizila kwambili za mmene anali kumvelela , m’malo moganizila za mmene angapelekele ulemelelo kwa Yehova . Yesu asanakwele kumwamba atumwi ake anamufunsa kuti : “ Ambuye , kodi mubwezeletsa ufumu kwa Isiraeli pa nthawi ino ? ” Kuposa kale , masiku ano pali zinthu zambili zimene zingatisokoneze . N’cocitika citi cimene cionetsa kuti Asa anali kudalila Mulungu ? Mwacibadwa , Sara anacita mantha ndipo anafuna kukana . Kodi Akristu ofikapo amapindula bwanji ndi cidziŵitso colongosoka ? Caciŵili , Baibo siikamba kuti Yesu kapena wophunzila wake aliyense anali kukondwelela Khrisimasi . Yesu anaseŵenzetsa thupi limene Mulungu anamukonzela pokwanilitsa nchito imene iye anam’patsa . Yesu anati : “ Ndiyenela kukalengeza uthenga wabwino wa ufumu wa Mulungu kumizinda inanso , cifukwa ndi zimene anandituma kudzacita . ” Komabe , kuwonjezela pa kuyamikila ufulu wathu wamtengo wapatali umenewu , tiyenelanso kupewelatu kuuseŵenzetsa molakwika . Cikhulupililo n’cofunika kwambili . Ndiye cifukwa cake kupitila m’Baibulo , Yehova watipatsa zitsanzo zambili pankhani ya cikhulupililo . Zinthu zimene zikucitika padzikoli zikuonetsa kuti ulosi wa m’Baibulo ukukwanilitsidwa ndiponso kuti mapeto a dongosolo loipali ayandikila . Tiyeni tikambilane zitsanzo zoŵelengeka . 4 : 18 ; Akol . 1 : 21 ) M’kupita kwa nthawi , ena amazindikila kuti analakwitsa , ’ ndipo amasankha kubwelela ku gulu la Yehova ngakhale kuti sicikhala capafupi . Mungatengele bwanji citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wodzicepetsa ? Zinthu zimene Bezaleli ndi Oholiabu anapanga zitapezeka masiku ano , zingaikidwe m’malo apamwamba kwambili osungilako zinthu zakale , ndipo anthu ambili angacite nazo cidwi kwambili . pangano la wansembe monga Melekizedeki . Kapena bwanji ngati sitili mbali ya gulu la anthu amene anawalembela cofalitsaco ? “ Kuika maganizo pa zinthu za mzimu ” sikutanthauza kuti basi munthu lomba waleka na kuganiza koma kumangolota zinthu zauzimu paliponse yayi . Mu nthawi ya Mose , akatswili ophika mkate anali kuphikila Aiguputo mikate ndi makeke osiyanasiyana . 110 : 3 ; Yes . 52 : 7 ) Kodi mungacite ciani kuti mugwile nao nchito yosangalatsa imeneyi ? ( b ) Tikambilana ciani m’nkhani ino ? N’ndani amene Yehova anali kudzagwilitsila nchito kutsogolela anthu Ake pansi pa utsogoleli wa Khiristu ? “ Mulungu ndiye cikondi . ” Malangizo amene ali m’Baibo ni ocokela kwa Mulungu ndipo mudzapindula ngati muwatsatila . Kodi iye amaona kuti utumiki umenewu ni wabwino ? Umaphatikizapo makhalidwe anu , zimene mumakhulupilila , komanso zocita zanu . Ngati mwasankha kuŵelenga Baibulo lomasulidwa bwino , mungatsimikizile kuti muŵelenga Malemba ogwilizana kwambili ndi zolemba zoyambilila . ( Mlal . 7 : 20 ) Mtumwi Paulo nayenso anakamba kuti : “ Onse ndi ocimwa ndipo ndi opeleŵela pa ulemelelo wa Mulungu . ” Caka ciliconse , ndimakhulupilila kwambili mfundo zimenezi , ndipo cidalilo canga cakuti tilidi ndi coonadi calimbilako . ” 7 : 13 , 14 . 2 : 15 - 17 ) Tisalole “ cinyengo camphamvu ca cuma ” ndi “ nkhawa za m’nthawi ino ” kulepheletsa banja lathu ‘ kugwila mwamphamvu moyo weniweniwo ’ m’dziko latsopano lolungama la Mulungu . — Maliko 4 : 19 ; Luka 21 : 34 - 36 ; 1 Tim . Iwo anali ndi bizinesi imene inali kuyenda bwino m’dziko la Australia . Komabe , anasiya bizinesi imeneyo kuti ayambe utumiki wa nthawi zonse . Kodi pali zimene zam’citikila ? Macaputala ndi mavesi amenewa ndi othandiza , koma zimakhala bwino kwambili kuŵelenga nkhani yonse n’colinga cakuti timvetse uthenga wocokela kwa Mulungu . Anthu ake ni Sebina , amene anakhalako m’nthawi ya Mfumu Hezekiya , ndi Graham , m’bale wa m’nthawi yathu ino . Cifukwa ciani ? Kuganizila mphoto imene tikuyembekezela n’kofunika ngako , kaya tili na ciyembekezo cokalandila moyo wosafa kumwamba kapena codzakhala na moyo wosatha pano padziko lapansi . Angasinthe zinthu zina kuti nkhaniyo ioneke kukhala yoona . 2 : 1 - 4 ) Cozizwitsa cimeneci cinapeleka umboni wosatsutsika wakuti Yehova anali kucilikiza gulu lake latsopano lopangidwa ndi ophunzila a Kristu . Ngakhale n’conco , Samueli analimbitsa cikhulupililo cake - cake kwa Yehova , ndi kucita zinthu zokondweletsa Atate wake wakumwamba . ( Miy . Mwina Adamu anaganiza kuti “ tsiku ” limeneli ndi la maola 24 . Kumbukilani kuti ubwenzi wathu ndi iye uli monga wa tate ndi ana . ( Sal . Ife tonse , acinyamata ndi acikulile , tikhale na “ zocita zambili nthawi zonse mu nchito ya Ambuye . ” — 1 Akor . Nayenso Sara anali kugwila nchito yake mwakhama . Ngakhale kuti ifeyo sitingacite zozizwitsa , tingathe kuphunzitsa anthu Mau a Mulungu ouzilidwa . M’bale Russell ndiye anali pulezidenti wa bungwelo . * Iye anali kukonda kwambili kuphunzila Baibo , ndipo mopanda mantha anavumbula kuti ciphunzitso ca Utatu komanso cakuti moyo sumafa n’zabodza . Mfumu Agripa analemba maiko amene mafumu aciyuda anali kulamulila kuphatikizapo madela akutali monga Mesopotamiya , kumpoto kwa Africa , Asia Minor , Girisi , ndi zilumba za pa nyanja ya Mediterranean . Ngakhale kuti anabwelela ku United States , kutumikila ku Ghana kunawathandiza kuti aziika patsogolo zinthu za Ufumu . Amathawa ngati mthunzi ndipo sakhalaponso . ” — Yobu 14 : 1 , 2 . N’cifukwa ciani citsanzo ca mkazi wamasiye n’colimbikitsa ? ( Yeremiya 5 : 31 ) “ Ambili adzati kwa ine pa tsiku limenelo , ‘ Ambuye , Ambuye , kodi ife sitinalosele m’dzina lanu , ndi kutulutsa ziwanda m’dzina lanu , ndiponso kucita nchito zambili zamphamvu m’dzina lanunso ? ’ ( Mat . 4 : 4 ) Akulu angawathandize mwa kuwapezela mabuku a m’citundu cawo ndi kupeza abale amene amakamba citundu cawo . Koma bwanji ngati sakukumvelani ? Muzilalikila mwakhama ( Miy . 27 : 2 ) M’malo mwake , tidzayesetsa kuona zabwino mwa abale ndi alongo athu , ndi kuwayamikila pa makhalidwe ao abwino , maluso ao , ndi zimene akwanitsa kucita paumoyo wao . ( Miy . Mwinanso , ngati mumacita khama kukonzekela nkhani zanu za pamsonkhano koma mulibe cidwi coyeletsa Nyumba ya Ufumu , mungadziikile colinga kuti muzigwilitsila nchito malangizo opezeka pa Aroma 12 : 16 . — Ŵelengani . Nanga n’ciani cinamuthandiza kupilila ? Kodi kulambila koona kumatithandiza bwanji kukhala acimwemwe ? Ponena za Aramagedo , ulosi wa m’Baibulo umati : “ ‘ Yehova akufuna kuimba mlandu mitundu ya anthu . Conco , malile ni ofunikila kuti tonse tisangalale na ufulu weni - weni . Iwo sangatithandize kapena kutivulaza , cifukwa ku Manda “ kulibe kugwila nchito , kuganiza zocita , kudziŵa zinthu , kapena nzelu . ” Cikondi cinali kudzakhala cizindikilo ca ophunzila oona a Yesu , komanso cinali kudzawathandiza kukhala ogwilizana . — Yoh . Cotulukapo cake n’cakuti , anapeza madalitso ambili , ndi ciyembekezo ca tsogolo lowala . Coyamba , tiyenela kuyesetsa kukhala ndi makhalidwe amene Paulo anakamba amene ni kudzicepetsa , kufatsa , kuleza mtima , ndi cikondi . Kodi Yehova samaona zimene zicitika ? Kudzicepetsa kumayamba ndi kuzindikila malo athu m’makonzedwe a Mulungu . Tiyeni tione zimene tingaphunzilepo pa cikhulupililo ca Yosefe . Mulungu sindiye amacititsa zinthu zoipa . Conco , molimba mtima anakamba na Abulahamu mosapita m’mbali . Mzimu wa Mulungu umatithandiza kuti tikhale gulu la abale ogwilizana padziko lonse . — Ŵelengani 1 Yohane 4 : 20 , 21 . Koma pambuyo pa “ masiku atatu ndi hafu , ” mboni ziŵili zimenezi zidzaukitsidwa . Ndipo zimenezi zidzadabwitsa anthu onse oona . — Chiv . Aliyense amene wasiya nyumba , abale , alongo , abambo , amayi , ana kapena minda cifukwa ca dzina langa adzalandila zoculuka kwambili kuposa zimenezi , ndipo adzapeza moyo wosatha . ” ( Mat . N’cifukwa ciani Baibo imayelekezela cilungamo na codzitetezela pacifuwa ? Yesu sanakalipe ndi zimenezo . Nafenso Akristu tingapindule ndi Cilamulo cimene Yehova anapeleka . Popeza tsopano ali na mwayi wogwilizana nafe , kodi sitingawathandize kuti asakhale ngati alendo pakati pathu ? Tidzakambilana zimenezi m’nkhani yotsatila . Motelo , pitilizani kukulitsa cipatso ca mzimu wa Mulungu , makamaka kuleza mtima . Cacisanu , n’kutheka kuti munasiya nchito imene inali kukudyelani nthawi yotumikila Yehova , ndipo munaona mmene Mulungu anakwanilitsila lonjezo lake lakuti : ‘ Sindidzakutaya ngakhale pang’ono . ’ Kodi mwaona kuti zizindikilo zonse zinai zimene zafotokozedwa m’nkhani ino ndi umboni wooneka ndi maso ? Paulo anagwila mau a Habakuku akuti : “ Wolungama adzakhala ndi moyo mwa cikhulupililo cake . ” Iye anali kutumikila mwakhama pofuna kupititsa patsogolo coonadi . David : Ndinabadwa m’caka ca 1945 , m’dziko la Shropshire , ku England . ( Aefeso 3 : 20 ) Atumiki a Yehova amacita zimene angathe kuti acite cifuno ca Mulungu , koma amadziŵa kuti zinthu zina sangakwanitse . Ŵelengani Chivumbulutso 19 : 7 . Cinanso , ise tonse tiyenela kukhala na colinga colandila aliyense amene wabwela pa misonkhano . Panthawi ina , anatitumanso kukacita nchito yoyang’anila cigawo , ndipo tinali na mwayi wodziŵana ndi abale na alongo osiyana - siyana m’dziko la Ireland . Pokamba za munthu amene “ akuyenda mosalakwitsa zinthu , ” wamasalimo anati : “ Sanena misece ndi lilime lake . Sacitila mnzake coipa , ndipo satonza bwenzi lake lapamtima . ” — Sal . Monga mmene katswili wina anakambila , tikakhala mabwenzi ake , iye “ amationa kukhala ofunika kwambili na kutikonda . ” Zofalitsa za Acinyamata . A Yohane : Eee ! Nikaona mmene Yehova akuyendetsela zinthu , cikondi canga pa iye cimakulila - kulila . ” Kuwonjezela pa kuseŵenzetsa nyambo , Satana amatiyofya kuti ticite zinthu zosakhulupilika pamaso pa Yehova . N’cifukwa ciani mnyamatayu anasankha utumiki umenewu ? ( b ) Fotokozani mmene Yehova anathandizila mlongo wina . M’dziko la Satanali muli zinthu zambili zokopa monga zovala , zakudya , zakumwa , zosangalatsa , na zina zambili . Koma panopa , ndapeza gwelo labwino kwambili la nzelu zonditsogolela . Macaputa amenewo amatithandiza kudziŵa mmene Yehova angatikhululukile . ( 2 Mafumu 20 : 1 - 7 ) Koma mapemphelo ambili sanali kuyankhidwa mwa njila imeneyi ngakhale m’nthawi za m’Baibulo . Makhalidwe abwino ali monga kampasi yodalilika , angathandize mwana wanu kuyenda panjila yoyenela Kodi kukonda Yehova kumatanthauzanji ? ( Mat . 3 : 16 , 17 ) Ngakhale kuti Yesu ni Mwana wa Mulungu , Yehova anakondwela poona kuti iye wasankha kudzipatulila kuti acite cifunilo cake . Olo kuti ena sakamba mau amenewa ndendende , amakhalabe atalumbila pamaso pa Mulungu . Kodi kale zofalitsa zathu zinali kufotokoza bwanji fanizo la anamwali 10 ? Nanga zotsatilapo zinali zotani ? Iye akumuuza kuti : “ Kale kwambili , Mulungu anapanga dziko lapansi ndi zonse zimene zilimo . Tikaona anthu akuvutika na zotulukapo zoipa za chimo la Adamu , timawamvela cifundo ndipo timafuna kuwathandiza . 5 : 21 , 22 , 27 , 28 ) Kuti tiphunzitse bwino cikumbumtima cathu , tiyenela kulola mfundo za Mulungu kutitsogolela . Mlongo wina amene tsopano akutumikila pa Beteli ku Brooklyn , anakumbukila thandizo limene analandila pamene anali kucita upainiya . Iye anati : “ Mlongo wina amene anali ndi galimoto anandiuza kuti , ‘ Nthawi iliyonse mukasoŵa wolalikila naye muzinditumila foni kuti tipite limodzi . ’ 17 , 18 . ( a ) Mungalione bwanji dzanja la Yehova pa umoyo wanu ? 1 : 9 - 11 ) Kodi si citsanzo cabwino kwa ife ? Koma Yehova ndiye ananithandiza kwambili . Pamene tinali kucoka , m’delali munali mutakhazikitsidwa mipingo iŵili ing’ono - ing’ono . Thanzi lathu . — Salimo 37 : 8 ; Miyambo 17 : 22 . N’nasiyanso makhalidwe abwino amene n’naphunzila nili mwana . Kupemphela kwa Yehova ndi kuŵelenga Baibulo kwandithandiza kukhala ndi maganizo oyenela . ” — Mlaliki 9 : 11 ; Salimo 145 : 18 ; 2 Akorinto 4 : 8 , 9 , 16 . Khalanibe Okhulupilika ku Ufumu wa Mulungu Popanda dzuŵa , padziko lapansi sipakanakhala camoyo ciliconse . Baraki anathamangitsa asilikali a Sisera mpaka kukafika ku Haroseti , dela limene linali pamtunda wa makilomita 24 . Ndipo n’zoona kuti ngati sathila petulo , galimotoyo ingaleke kuyenda . Baibulo limati : “ Iye akudziŵa bwino mmene anatiumbila , amakumbukila kuti ndife fumbi . ” N’ciani cimene cinapangitsa ana a Nowa kukhala citsanzo cabwino kwambili ? Mwacitsanzo , popeza Nowa anali ‘ kuyenda ndi Mulungu woona , ’ anapewa kugwilizana ndi anthu osaopa Mulungu . Kodi angelo anam’thandiza bwanji Mose ? ( Aroma 13 : 6 ) Koma kwina makonzedwe amenewa kulibe . Pophika cakudya cimeneci anali kuikako nandolo , tomato , anyenzi ndi zinthu zina zokometsela . Mfundo za m’nkhani ino zimagwilanso nchito kwa aja amene afunitsitsa kukhala atumiki othandiza . Tsiku lina madzulo , tinakambilana za kutulutsiwa kwa kabuku kakuti God’s Way Is Love , kamene anakakonzela maka - maka anthu a ku Ireland . Ni malangizo a mphamvu ati amene Petulo anapeleka ? Kodi n’kulakwa kufunsa funso limeneli pa nkhani ya pemphelo ? Na ise ngati timaidziŵa bwino nchito yathu mofanana ndi Yesu , tidzapewa kucilikiza ngakhale mwakacetecete magulu andale omenyela ufulu wodzilamulila . Kodi pali umboni wa zinthu zakale wotsimikizila nkhani za m’Baibo ? Kupitila mwa Mose , Yehova analamula Aisiraeli kuti azikaonekela pamaso pake , pa zikondwelelo zitatu za pa caka . ( b ) Nanga n’cifukwa ciani sitiyenela kubwezela coipa ndi kusunga cakukhosi ? Mizuho , amene anacokela ku Japan anati : “ Ine na mwamuna wanga , Sachio , takhala tikulakalaka kukatumikila m’dziko limene kuli ofalitsa ocepa . 16 : 1 - 5 ) Iwo mosabisa anatsutsa Mose ndi kukanilatu utsogoleli wake wopatsidwa ndi Mulungu . Kuti timvetse bwino fanizo la nkhosa ndi mbuzi , coyamba tifunika kudziŵa zinthu zitatu zochulidwa m’nkhaniyi . Tifunika kudziŵa anthu amene akuchulidwa , nthawi imene kuweluza kudzacitika , ndiponso cifukwa cimene cidzacititsa kuti ena akhale nkhosa kapena mbuzi . ( Danieli 1 : 3 - 5 , 13 ) Zikuoneka kuti Danieli anali ndi udindo wapamwamba kwambili ku Babulo kuposa umene akanakhala nao ku Isiraeli . Kugwilizana ndi okhulupilila anzathu kungatithandize kuganizila za dziko latsopano ( Onani ndime 19 ) Iye anati : “ Mwana wathu Don atabadwa , ine ndi mwamuna wanga tinali kuseŵenza kudziko lina , ndipo ndinali nditayamba kuphunzila Baibulo . Koma mosasamala kanthu za njila imene tingaseŵenzetse pokonzekela , tifunika kuŵelenga malemba amenewa mosamala na kuwasinkhasinkha . Mwinanso anzanu kunchito amakunyozani cifukwa copempha chuti kapena kulephela kusewenza ovataimu kuti mukacita zinthu zauzimu . Kodi mphunzitsi afunika kucita ciani ? 3 : 11 ; Agal . Zinthu monga magazini okopa , mawailesi , mafilimu , ndi ma TV , zinali zofala kwambili . Tinakondwela kwambili kupezeka pa msonkhano wathu woyamba pambuyo pa miyezi 5 . Umacititsanso kuti azingofuna kukhutilitsa zilakolako zawo za thupi . Anthu ambili amene anali na njala ya coonadi ca m’Baibo anathaŵila ku maiko ena kumene chechi siinali na mphamvu zopitilila . Davide atapha Goliyati na kupatsidwa mwana wamkazi wa Mfumu Sauli kukhala mkazi wake , anakamba kuti : “ Ndine yani ine , ndipo abale anga , anthu a m’banja la bambo anga ndani mu Isiraeli monse muno kuti ndikhale mkamwini wa mfumu ? ” ( 1 Sam . Mimbulu imeneyi m’zovala za nkhosa inayamba ‘ kuononga cikhulupililo ca ena . ” 123 : 1 . Tsopano , ngakhale kuti papita zaka zambili , ndikusangalala kuti pamene ndinali mtsikana ndinatumikila Yehova . 18 Tumikilani Yehova ndi Mtima Wathunthu Seŵelo imeneyi inaphatikiza kanema , mapikica , ndi mau ofotokoza mbili ya munthu kucokela pamene analengedwa mpaka kumapeto kwa zaka Cikwi . Kuti Aisiraeli aonetse kuti anali kulemekeza wopatsa moyo , anali kufunika kupewa kucita zinthu zimene zikanaika moyo wa mnzawo paciopsezo . ( Numeri 21 : 5 ) Potsilizila pake , mkatewu wocokela kumwamba unakhala wonyansa kwa io . — Salimo 105 : 40 . MKATE WAMOYO Mlongo wina analemba kuti : “ Tsopano ndili ndi mipata yambili yogaŵila Mau a Mulungu kwa anthu a m’gawo lathu . 29 : 7 ) Koma pa nthawi imodzi - modziyo anawalamula kuti akhale odzipeleka kwa iye yekha cabe . 8 : 10 ) Ciŵelengelo conse ca anthu a m’pangano latsopano ndi 144,000 . Ndipo anthu amenewa amapanga mtundu watsopano umene ndi “ Isiraeli wa Mulungu , ” kapena kuti Isiraeli wa kuuzimu . — Agal . 5 : 28 , 29 ) Mulungu walonjeza kuti “ adzameza imfa kwamuyaya ndipo Yehova , Ambuye Wamkulu Koposa , adzapukuta misozi pankhope zonse za anthu . ” Onani kuti aŵili pa mafunso amenewa , akamba za kuteteza cikhulupililo cathu molimba mtima ndi kusatengela zocita za anzathu . Danieli 4 : 20 - 36 . Tinalinso kulalikila mosamala kwa akaidi ena , ndipo ena mwa iwo anakhala Mboni za Yehova . Mkazi wanga amadwala - dwala . ( 2 Akor . Iye anayeletsa kacisi , anapempha Mulungu kuti akhululukile anthu ake , ndiponso anaononga mafano onse amene anali m’dzikolo . [ Mau apansi ] Ofufuza ena anafotokoza kuti abale ake a Yosefe anaona kuti mphatso imene bambo wao anapatsa Yosefe inapeleka umboni wonena kuti iye anali kufuna kuti mnyamatayo alandile ufulu wa mwana woyamba kubadwa . Kodi Mudzalandila Mphatso ya Mulungu Yopambana Zonse ? 1 : 10 . Ndipo pamene Paulo anali kulemba kalata kwa abalewo , n’kuti ali paukaidi wosacoka panyumba ku Roma . Pali zinthu zina zimene zingatilepheletse kutumikila bwino , zinthu monga maudindo a m’banja , kudwala , kapena mavuto ena . ▪ Khalani Wodzicepetsa ndi Wacifundo Monga Yesu C.E . , gawo lao linakula kwambili cifukwa anayamba kulalikila ngakhale kwa anthu osadulidwa . N’cifukwa ciani acikulile afunika kuphunzitsa acinyamata ? ( 1 Timoteyo 2 : 1 , 2 ) Ndipo anthu ena akaticitila zinthu zopanda cilungamo , tingapemphe akuluakulu a boma kuti atithandize . Panthawiyo , anthu okhulupilika adzakhala atapeleka umboni wakuti anthu akhoza kucilikiza ulamulilo wa Mulungu molimba mtima . ( Yes . Monga mmene udzu umakulila m’munda , mkwiyo ungakule mumtima ngati sitiyesetsa kuucotsa . Msuweni wa amai anga anali wansembe ndiponso mphunzitsi pa sukulu ya Katolika . Conco , popeza kuti Malemba sakamba kuti mizinda yothaŵilako inali kuimila zinthu zina zam’tsogolo , nkhani ino na yotsatila , zidzafotokoza kwambili zimene ise Akhristu tiphunzilapo pa makonzedwe a mizinda yothaŵilako . Muganiza bwanji , kodi zinali zotheka kuthandiza Gavin ? Tsopano io adzapezeka ndi mlandu . ” ( Hos . Nkhani ya Asa iyenela kutilimbikitsa kudzifufuza pa zocita zathu . ( Yoswa 3 : 15 - 17 ; 5 : 10 ) Monga mmene tanenela , mumzinda wa Yeriko munapezeka zakudya zambili . Izi zionetsa kuti mzindawo unaonongedwadi m’kanthawi kocepa monga mmene Baibulo limanenela . N’ciani cinapangitsa kuti mkulu wacikhristu wokhwima mwauzimu ameneyu acite zinthu zimene zikanayambitsa magawano mumpingo ? Baibo imati : “ Ngati munthu akukonda Mulungu , ameneyo amadziŵika kwa Mulungu . ” Pofuna kutithandiza kumvetsetsa mmene munthu wauzimu amakhalila , mtumwi Paulo anafotokoza kusiyana pakati pa “ munthu wauzimu ” na “ munthu wakuthupi . ” Pafupifupi zaka 3,000 zapitazo , mneneli Eliya anaitana Elisa amene anali wacinyamata kuti akhale mtumiki wake . 6 Tsopano , timakondwela kwambili tikaona ofesi ya nthambi ku Lilongwe imene inamalizidwa m’caka ca 2000 ndiponso Nyumba za Ufumu zatsopano zoposa 1,000 zimene zamangidwa m’dziko lonse la Malawi . Komabe , kwa zaka zambili colinga canga cakhala kupitilizabe kumvela amene akutsogolela . ” Ndiyeno ndinagula tuŵana twa nkhuku 40 . Ndithu ndikuthandiza . Ndiyeno , iye anam’tenga kukhala mwana wake . ( Backgrounds of Early Christianity ) Ayuda sanali kukamizidwa kumenya nawo nkhondo . Ali mwana , mosakayikila anali kuseŵela ndi kucita zosangalatsa . ( Mateyu 7 : 13 , 14 ) Inde , tsogolo lanu lidalila pa zosankha zimene mumapanga . Ndi zitsanzo ziti zamakono zimene zionetsa kuti Yehova amavomeleza ziphunzitso zomveka bwino ? Kodi mwaona zimene lemba la Zekariya 5 : 3 , 4 lakamba ? Lakamba kuti “ tembelelo . . . lidzaloŵa m’nyumba ya munthu wakuba ndi . . . kukakhala m’nyumba mwake n’kuwonongelatu nyumbayo . ” Malipoti ocokela ku maofesi ena a nthambi amaonetsa kuti m’maiko ena , anthu sakonza zinthu zoonongeka pa Nyumba za Ufumu . Caka ciliconse , Mboni za Yehova padziko lonse zimasonkhana kuti zikumbukile imfa ya Yesu . ( Miyambo 23 : 20 ; 2 Akorinto 7 : 1 ) Kutsatila malangizo a m’Baibulo kungatithandize kuteteza thanzi lathu . Nkhondo , njala , matenda , ndi zinthu zina zimene zimaphetsa anthu zidzaculuka . 16 : 1 - 3 . Tifunika kukumbukila kuti mwana aliyense ali na cibadwa cake , ndipo ana amakula mosiyana - siyana . Funso limenelo n’lomveka . Koma timadziŵa kuti ndi udindo wathu ‘ kulankhula ndi anthu oipa ndi kuwacenjeza kuti asiye njila zao zoipa ndi colinga cakuti akhalebe ndi moyo . ’ Tifunika kuphunzila Mau a Mulungu ndi kuwagwilitsila nchito . M’Baibo muli zitsanzo zoticenjeza zimene zionetsa kuti nsanje ingatilepheletse kukalandila mphoto . Cidzaniŵaŵa maningi ngati sudzayenda , ” anatelo Amayi . Atadziŵa kuti sadzabala m’dongosolo lino la zinthu , zinamupweteka kwambili mumtima . Nthawi zina , akazi ena angakonde kuti Yehova aloŵelelepo pa nkhani inayake monga anacitila kwa Sara . Acibalewo anagwilizana zakuti acite mwambo wogona pamalilo koma ndinawaletsa , ndipo ndinawauza kuti ngati aumilila , sayenela kucitila pa nyumba panga mwambowo . ( Salimo 37 : 28 ) Ngakhale kuti Mulungu sanalekelele cimo la dala la munthu woyamba , iye sanaweluze kuti anthu onse apitilize kuvutika ndi kufa cifukwa ca kusamvela kwa munthu mmodzi . N’cifukwa ciani tinganene kuti Tsiku Lophimba Macimo silinali tsiku la mwambo cabe ? ( b ) Kodi Yehova pang’onopang’ono anaulula ciani ponena za mbeu ya mkazi ? ( Miyambo 24 : 10 ) Koma Yehova “ amapeleka mphamvu kwa munthu wotopa , ndipo wofooka amam’patsa nyonga zoculuka . ” Poyamba , Pakistan inali kuphatikizapo West Pakistan ( imene lomba ni dziko la Pakistan ) na East Pakistan ( imene lomba ni dziko la Bangladesh ) . Zomvetsela zambili monga zimenezi zimapezeka pa webusaiti ya jw.org . ( Mac . 1 : 6 - 8 ) Kupitila m’nchito yolalikila Ufumu , anthu zungulile dziko lapansi ali ndi mwayi wophunzila za dipo ndi kukhala nzika za Ufumu wa Mulungu . Zili conco kaya ni pa nkhani ya makhalidwe kapena kulambila . Ndinali kufuna kuona zimene Mabaibulo ena amakamba pa lembali . Ndinayang’ananso dzina la Mulungu mu dikishonale . ZIMENE MAU A MULUNGU AMAPHUNZITSA : Mulungu sanangotipatsa Baibulo kenako n’kungotiiŵala . Patapita zaka zambili , Yehova anacha Aisiraeli kuti ni Mboni zake ndipo anawauza kuti : “ Ine sindinasinthe . Kumaiko ena , kusunga ndevu zodulila bwino - bwino n’kololeka , ndipo sikulepheletsa anthu kumvela uthenga wa Ufumu . Tikamapezeka pamisonkhano , timaonetsa kuti tifuna kumvela Yehova . Koma pamene anali kukumana ndi mavutowo , Yehova anali nao . 3 : 1 , 2 ) Kodi tiphunzilapo ciani pa nkhani zimenezi ? ( 2 Akorinto 11 : 29 ) Ngakhale kuti nilibe manja , nimaganiza na kukamba . Ena m’dzikoli amadziona kuti ni anzelu , ndipo amakamba kuti , “ Ningakhale na mfundo zabwino zoyendetsela umoyo wanga popanda kukhulupilila Mulungu . ” N’ciani cinathandiza Kyung - sook kupilila matenda oopsa ? Cifukwa coopa Yehova , io molimba mtima anakana kupha anawo . Izi zidzam’patsa mphamvu zokwanila kuti akwele phililo mpaka kukafika pamwamba . ( Onani cithunzi cili kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) N’cifukwa ciani sitiyenela kucita mantha kukambitsilana ndi anthu nkhani zovuta ? Ngakhale kuti n’zovuta ‘ kuleka kucita zosalungama , ’ n’ciani cimatithandiza kuleka kucita zimenezo ? Lembali limati : “ Khalanibe oganiza bwino ndipo khalani maso . Timaonetsa bwanji kukhulupilika kwathu kwa Yehova popanga zosankha zazikulu ? M’malo mwa nkhawa yosautsa maganizo , Mulungu anawathandiza kukhala na mtendele waukulu umene umaposa kuganiza kwaumunthu . Mwina iye anali kuganizila za mkazi wake , ana ake aakazi , mwana wake wamwamuna Metusela , kapena mdzukulu wake Lameki . Ndipo vuto la kusadziletsa likukulila - kulila . Thandizo limene anawapatsa , kuphatikizapo khama lawo lofuna kukwanilitsa zolinga zauzimu , zinawathandiza kupita patsogolo . Zinawathandizanso kuti asasoceletsedwe na dziko loipa la Satanali . Kodi Mulungu analenga anthu kuti azikhala kumwamba ? 128 : 1 - 6 ) Mwacitsanzo , Deuteronomo 28 : 4 imati : “ Cidzadalitsika cipatso ca mimba yako , cipatso ca m’dziko lanu , cipatso ca ziŵeto zako , ana a ng’ombe zako ndi ana a nkhosa zako . ” Ndiyeno anaŵelenga lemba limodzi la Salimo 83 : 18 . Ponena za Yobu , Satana anati : “ Tsopano tatambasulani dzanja lanu ndi kukhudza mnofu wake mpaka fupa lake , ndipo muona , akutukwanani m’maso muli gwa . ” Anthu ambili ndi otsimikiza kuti tafikadi m’nthawi yapadela . Nanga n’cifukwa ciani takamba conco ? Modzicepetsa , Yosefe anauza Farao kuti : “ Yemwe anene . . . ndi Mulungu osati ine ” Wathyola uta ndi kuduladula mkondo . Ndipo watentha magaleta pamoto . ” Mtumwi Paulo anauza Timoteyo kuti azisinkhasinkha mmene zokamba zake , khalidwe lake ndi zimene amaphunzitsa zimakhudzila anthu ena . Pambuyo pake , pamene anaona kuti angakwanitse kuphunzila Cimalagase , anakukila mu mpingo wa citundu cimeneci . Komanso , cingelezi ndi cimene amagwilitsila nchito ku Patterson , New York , pophunzitsa abale ocokela ku maiko osiyanasiyana . Tizikumbukila kuti iye amangoleza mtima koma amafunitsitsa kutithandiza . “ Cikondi cimene Khristu ali naco cimatikakamiza . . . Sitikanakhala pa mtendele ngakhalenso paubale wabwino ndi iye . . . . Kodi N’zoona Kuti Davide Anamenyana ndi Goliyati ? ( Aroma 1 : 3 ) Apa tingakambe kuti Baibulo limationetsa mizele iŵili yosiyana imene Yesu anabadwilamo . Pokamba na munthu amene afuna kukulembani nchito , kodi mudzamuuza kuti tsiku limodzi mkati mwa wiki iliyonse mumafunika kusonkhana ? Yesu anali kuwakonda ophunzila ake ndipo analinso wodzicepetsa . Mwacitsanzo , mnyamata anakamba kuti maso a wokondedwa wake anali monga “ maso a njiwa , ” kusonyeza kuti anali kukonda maso a mtsikanayo . ( b ) Mumamvela bwanji mukaganizila mwayi umene muli nawo wocilikiza pa nchito ya Ufumu ? Kugwila nchito molimbika kudzakuthandizaninso kukhala na mbili yabwino . ” — Reyon . Anthu amenewa sangakwanitse kucotsapo nkhondo , upandu , matenda , na umphawi . Tiyeni tikambilane mafunso atatu awa : ( 1 ) Ndi uthenga wanji womwe uli m’fanizo limeneli ? Ena mwa malamulowo anali acibadwa , koma anali malamulo ndithu . ( Afilipi 4 : 13 ) Ifenso tiyenela kupempha mzimu woyela tili ndi cikhulupililo cakuti Yehova adzayankha mapemphelo athu ocokela pansi pa mtima . — Salimo 10 : 17 . Iye ‘ anasautsika , ’ kutanthauza kuti anavutika mtima . Ndipo analibe mphamvu zolimbana ndi mavuto . Mungagwilitsile nchito nthawi yanu kumvetsela Baibulo pa CD , mabuku ofotokoza Baibulo , nkhani za onse , ndiponso masewelo . Kudziŵa mmene Yehova anacitila zinthu ndi atumiki ake kungatithandize kuona zofooka za anthu mmene iye amazionela . Iwo sayenela kuuza munthu wina kuti wadzozedwa ndiponso kuti azidya mkate ndi kumwa vinyo pa Cikumbutso . Koma ophunzila a ku Lusitara anapita kwa Paulo ndi kumuzungulila . Pambuyo pa ulamulilo wake wa zaka 1000 , Yesu adzapeleka Ufumu wake m’manja mwa Yehova , kuti ‘ Mulungu akakhale zinthu zonse kwa aliyense . ’ — 1 Akor . Kodi wacicepele angaonetse bwanji kuti ali na nzelu zomuthandiza kuti akapulumuke ? Ngati nyumbayo inali yolingana ndi manyumba amene ofukula zinthu zakale apeza mumzinda wa Uri , ndiye kuti Sara anasiya umoyo wabwino maningi . 2 , 3 . ( a ) N’cifukwa ciani Yehova anatifotokozela bwino kwambili za umoyo wa Yesu m’Baibulo ? Nanga Yehova afuna kuti ticite ciani ? Iye [ Yesu ] adzatumiza angelo ake ndi kulila kwamphamvu kwa lipenga , ndipo adzasonkhanitsa osankhidwa ake kucokela ku mphepo zinayi , kucokela kumalekezelo a m’mlengalenga mpaka kumalekezelo ena . ” ( Mat . Ena anali opembedza mafano , acigololo , amuna ogonana ndi amuna anzawo , akuba , zidakwa , ndi ena aconco . ( b ) N’cifukwa ciani mudzapezeka pa Mgonelo wa Ambuye ? Kapena kodi anthu ambili amakhulupilila cabe zimene amaona ? ( 2 Akor . Patapita masiku aŵili , ophunzila ake akuyang’ana kacisi mu Yerusalemu , mmodzi wa iwo anafuula kuti : “ Mphunzitsi , taonani mmene miyala ndi nyumbazi zikuonekela ! ” iye anapitiliza mwa kuyankha kuti : “ Mulungu adzatelo kudzela mwa Yesu Kristu Ambuye wathu . ” Nthawi zina , munthu amangosankha mwadala kucita zinthu zina m’malo mopita kumisonkhano . Koma mwamuna wina amene banja lake likuyenda bwino , dzina lake Kweku anati : “ Nthawi zonse ndimafunsa mkazi wanga ngati pali nchito imene ndingamuthandize . Kenako anauza Sauli kuti apite atamuthandiza kukonzekela udindo wake wamtsogolo . — 1 Sam . ( Yoh . 6 : 44 , 45 ) Pa anthu 1,000 alionse padziko lapansi , ndi munthu umodzi yekha amene ali ndi cidziŵitso colondola ca Baibulo , ndipo inu muli pakati pa anthu ocepawo . Tangoganizilani mmene iwo anasangalalila kumvetsela kapena kuŵelenga Mau a Mulungu m’citundu cimene anali kucimvetsetsa ! Gwen : Vuto lalikulu limene ndinali kufunikila kuthetsa linali kukhulupilila zamatsenga . Kodi Kukhala pa Mzela wa Makolo a Mesiya Kunadalila Kukhala Oyamba Kubadwa ? M’dziko lililonse , wansembeyo anafunsa Mboni za Yehova kuti , ‘ Kodi mukulalikila uthenga wotani ? ’ 16 : 14 , 16 . Tikacita zimenezo , tidzatha kupulumuka pamene Yehova adzapeleka ciweluzo kwa anthu amene amaphwanya mwadala malamulo ake . Komabe , ndimalalikila nthawi zonse . Mmodzi wa io anali Eliya . Zoonadi n’zakuti palibe aliyense amene amafuna kufa . Pitilizani kukhulupilila malonjezo a Yehova . Kucita zimenezi kudzakuthandizani kukhala wofunitsitsa kulalikila uthenga wabwino . Masiku ano , abale ndi alongo athu ambili apitilizabe kukhala okhulupilika . Conco , Terofimo anatsalila ku Mileto kuti apezeko bwino . Banja limenelo linatumiza makalata ku maofesi a nthambi anayi . Izo zidzaukitsidwa , kapena kuti zidzakhalanso ndi moyo padziko lapansi . — Yoh . Nthawi zonse tizipezeka pamisonkhano ya mpingo , ya dela ndi ya cigawo . ( Aheb . Mayiwo anali wofunitsitsa kuti akambilane zambili za m’Baibulo . Koma nitafeluka , anadziŵa ndipo anakhumudwa ngako . ( b ) Kodi anthu a Mulungu akhala akugwilitsila nchito motani cinenelo kuyambila panthawiyo ? Kuti munthu akhale ndi cikhulupililo colimba , ayenela kucita zambili osati kuŵelenga cabe Baibulo . Kuti amasulile Baibulo molondola , a Komiti Yomasulila Baibulo la Dziko Latsopano anatsatila mfundo zitatu zofunika izi : ( 1 ) Kulemekeza dzina la Mulungu ndi kulilemba m’Mau ake mofanana ndi mmene linalembedwela m’mipukutu yoyambilila . Motelo , kodi munthu angadziŵe bwanji kuti ayenela kudya zizindikilo kapena ai ? ( Yoh . 13 : 34 , 35 ) Ganizilani madalitso amene tili nao pokhala m’gulu lapadziko lonse la abale odzimana . 5 , 6 . Zambili mwa zinenelozo n’nali nisanazimvepo , koma n’nali wokondwa kudziŵa kuti magazini ambili - mbili anali kutumizidwa kumaiko akutali . Kodi kukhala paubwenzi ndi Yehova kumatithandiza bwanji kupewa ciwelewele ? Ndiyeno yesetsani kukonda zimene amakonda . M’bale Julian anati : “ Iye anali mwana wanga ndithu , koma khalidwe lake linapangitsa kuti tisamacite naye zinthu pamodzi . ” Atsogoleli azipembedzo a m’nthawi ya Yesu anakonza njila zakuti anthu aziwalemekeza na kuti azionetsa ulamulilo wawo . Mungaonetse bwanji kuti mumayamikila mphatso yopambana zonse imeneyi ? Yehova Anamucha kuti “ Bwenzi Langa , ” Feb . Kodi akuoneka ndi nkhope yacisoni ? ( b ) Mumamva bwanji mukaganizila za dipo ? Baibulo limatiuza mmene moyo padziko lapansi udzakhalila pamene sikudzakhala ukalamba , matenda ndi imfa . — Ŵelengani Yesaya 25 : 8 ; 33 : 24 ; Chivumbulutso 21 : 4 , 5 . Kodi tiyenela kukumbukila bwanji imfa ya Yesu ? 10 : 10 ) Koma kumbukilani kuti Paulo anakhala Mkhristu pambuyo poona Yesu m’masomphenya panjila . Mofananamo , ngati tikamba mosamala , timagwilitsila nchito lilime lathu kulemekeza Yehova ndi kulimbikitsa ena . — Salimo 19 : 14 . Tikamvela malangizo ake ndi kulapa , iye amatikhululukila “ ndi mtima wonse . ” ( Nyimbo 1 : 1 ) Koma m’nyimboyi , Solomo sanalembe maina a amene akulankhula . Banja lathu ni la mtundu wacikigizi ndipo timakamba cikigizi . Cikhulupililo cimaphatikizapo “ kudziŵa ” Mulungu monga munthu . 9 : 14 ) Zoona , umenewu ni uthenga wabwino umene tiyenela kuuzako ena . Stephen Langton asanabadwe , akatswili ena anali atayesepo kugaŵa Baibulo m’njila zosiyanasiyana kuti anthu asamavutike kupeza mbali imene akufuna . Tiphunzilapo ciani pa mafanizo opezeka pa Mateyu caputala 24 ndi 25 ? Iye anamupeza na matenda a manjenje . Zimene io amacita monga akazembe a Mulungu ndi Kristu zimapangitsa kuti anthu oona mtima akhale paubwenzi ndi Yehova ndi olambila anzao . — Ŵelengani 2 Akorinto 5 : 18 - 20 ; Yoh . 6 : 44 ; Mac . 13 : 48 . Kutumikila pa Beteli kwanipatsa mwayi woona bwino kukula kwa coonadi mu Philippines . Mwina , umu ndi mmene Abulahamu anaphunzilila za Yehova . ( Akol . 2 : 7 ) Kodi mumatsatila malangizo a gulu la Yehova amenewa ? ( a ) Tifunika kucita ciani kuti Mau a Mulungu atithandize pa umoyo wathu ? Nanga n’cifukwa ciani miting’i imeneyi inali yofunika kwambili ? N’cifukwa ciani tingakambe kuti ulamulilo wa Yehova si wopondeleza ? 5 : 22 ) Conco , n’zoonekelatu kuti oyang’anila oyendela ndi amene anali kuika abale pa udindo , osati atumwi kapena akulu ku Yerusalemu . “ Pitiliza kukhala wodzipeleka poŵelenga pamaso pa anthu , powadandaulila , ndi powaphunzitsa . ” — 1 TIM . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti ndi wolimba mtima ? Popeza nidziŵa bwino mmene cimvekela kukhala wolemala , nimatha kutonthoza ena amene sakwanitsa kucita zambili . Ganizilani zimene mungacite kuti muwonjezele utumiki wanu ( 1 Yohane 5 : 14 ) Koma , kodi zimenezi zitanthauza kuti Mulungu amayankha mapemphelo onse a olambila ake ? Iyai . Mtumwi Yohane anatanthauza kuti okana Kristu ndi anthu amene mwadala amafalitsa mabodza acipembedzo onena za Yesu Kristu ndi ziphunzitso zake Nanga ni mfundo za m’Malemba ziti zimene afunika kuganizila ? ( Mac . 2 : 5 , 44 - 47 ) Cikondi cimene Akhiristu aciyuda anaonetsa kwa Akhiristu ocokela ku malo osiyana - siyana , cinaonetsa kuti anali kudziŵa tanthauzo la mau akuti “ kuceleza , ” amene amatanthauza kukomela mtima alendo . Izi ndi zimene ophunzila ake anacita m’nthawi ya atumwi . Komabe , mfundo yake imagwilanso nchito kwa amene ali ndi ciyembekezo ca padziko lapansi . Anthu a Yehova amene anatsatila malangizo ake anadalitsidwa , mosasamala kanthu za njila imene anawalandilila . Kodi ‘ Mumamvetsa Tanthauzo la Malemba ’ ? Ganizilani zinthu zabwino zimene zimatulukapo munthu akaphunzila Baibulo . N’zoonekelatu kuti apa Yesu anali kuganizila zoti posacedwa apeleka moyo wake cifukwa ca mtundu wa anthu . Ine na mwamuna wanga tikanakhala kuti sitinali kucita zinthu mogwilizana , sembe tili monga anthu aŵili amene akhala cabe m’nyumba imodzi , ndipo sakambilana popanga zosankha zikulu - zikulu . ” — Alexandra . 55 : 22 ) Mau otonthoza a Paulo ni ozikidwa pa mfundo ziŵili zofunika za coonadi . Motelo , tifunika kupatula nthawi yoŵelenga Baibulo , kusinkhasinkha kuti tilimvetsetse , ndi kutsatila malangizo ake . ( Genesis 6 : 9 ) Conco , kaya tikumane ndi mavuto azacuma panthawi ino kapena mtsogolo , citsanzo ca Paul ca kukhala ndi cikhulupililo komanso kugwilitsila nchito nzelu zopindulitsa cimatiphunzitsa zinthu zofunika kwambili . ( 2 Mbiri 16 : 9 ) Mwacitsanzo , iye anaona zabwino zimene Mfumu Yehosafati ya Yuda inacita . Kodi m’Baibulo muli nkhani ina imene simumvetsetsa ? Mau athu acifundo . Njila ina yotetezela ufulu wathu ni kudalila Yehova , na kum’lola kuti azitithandiza kusalumpha malile amene anatiikila . Barr , amene pambuyo pake anatumikila m’Bungwe Lolamulila . Natalia , mai wa ana aŵili anati : “ Taona kuti cofunika kwambili ku banja lathu ndi kusintha - sintha nkhani zokambilana . ” Koma ifenso tiyenela kuthandiza abale athu ndi kuwapemphelela . Masiku ano , mzinda umenewo ni matongwe okha - okha . 14 Kodi Mumalemekeza Buku Lake la Yehova ? N’cifukwa ciani tifunika kukhala acifundo nthawi zonse ? Ndani adzandipulumutse ku thupi limene likufa imfa imeneyi ? N’zotheka Banja Lanu Kukhala Lacimwemwe Conco , iye amakamba zimene akufuna mwa kuyang’ana kwambili dzanja limene waona kuti ndi loyenela . Yesu anadziŵa kuti kulandila alendo n’kofunika kwambili . Cilamulo cinathandiza anthu a Mulungu kusaiŵala kufunika kwa cilungamo posamalila nkhani za m’banja na zina . Nanga n’cifukwa ciani waiteteza kuti ikhalepobe mpaka lelo ? Nthawi ina ndinapeza ndalama zokwanila $ 10,000 pa tsiku limodzi lokha . 55 : 12 - 14 . William Malenfant ( Sal . 147 : 3 ) Ndithudi , Yehova amasamalila anthu amene akumana ndi mavuto . Amawathandiza mwakuthupi ndi kuwalimbikitsa . Zaka ziŵili Yesu asanafe ndi kupeleka nsembe ya dipo , anaphunzitsa ophunzila ake kupemphela kuti : “ Atate wathu wakumwamba , dzina lanu liyeletsedwe . Ana amadalila makolo ao kuti awathandize ndi kuwateteza . ( Yohane 3 : 36 ) Kodi kukhulupilila kumatanthauza ciani ? ( Yesaya 43 : 23 ) Cotelo , tikamamvela lamulo lake lakuti tizipezeka pamisonkhano , timaonetsa kuti timamukonda ndi kuti timakhulupilila kuti iye ndiye ali ndi ufulu wotiuza zocita . Kodi kukhala na “ cilakolako ca kugonana ” cosaletseka kumabweletsa mavuto anji ? ( Yohane 3 : 16 ) Tikalakwa , tiyenela kupempha Yehova kuti atikhululukile . Tingacite bwanji zimenezi ? Pitilizani kuwalanga moleza mtima mwa kuwatsogolela , kuwaphunzitsa , ndi kuwaongolela . Pamene Petulo anali kuyenda pa Nyanja ya Galileya , iye anayamba kucita mantha . 1 : 9 ) Iwo anacitila umboni za Yehova ndi Yesu “ mu Yerusalemu , ku Yudeya konse ndi ku Samariya , mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ” — Mac . Ndipo mumafika pomuyandikila kwambili Yehova Ngati munthuyo ni wokamba - kamba , ndipo imwe ndimwe wa zii , ganizilani mmene zimakhalila zosavuta kwa iye kuyambitsa makambilano muulaliki . ( 1 Pet . 2 : 21 ) Popeza ndife opanda ungwilo , kodi n’zotheka kutsatila citsanzo cangwilo ca Yesu ? Koma mukudziŵa kuti mukapitiliza kuyenda , mufika kumapeto kwa ngalandeyo , ndipo muyambanso kuona kuwala . Cikondi ceniceni cinali cosoŵeka ngakhale m’nthawi ya Mfumu Solomo . 13 : 7 ; Mat . NYIMBO : 133 , 135 Nkhondo za pa dziko lonse komanso zing’ono - zing’ono , zapha anthu osaŵelengeka kuyambila 1914 . Ndiyeno “ khamu lalikulu ” la nkhosa zina lidzapulumuka cisautso cacikulu . — Chiv . Pambuyo pakuti Mfumu yatsopanoyo yacotsa Satana ndi ziwanda zake kumwamba , Yehova analamula Yesu kuti ayendele ndi kuyenga otsatila ake mwakuuzimu padziko lapansi . Zaka zapitazo , mpainiya wina wa ku Japan , dzina lake Kazuhiro , anakomoka ndipo anapita naye ku cipatala . M’nkhaniyi , tidzakambilana zimene zinacititsa kuti munthu wokhulupilika Mose ataye mwayi woloŵa m’Dziko Lolonjezedwa . Conco , kuti mupindule kwambili poiphunzila , muyenela kukhala na maganizo monga a mwana , amene amakhala wokonzeka kuphunzila kwa tate wacikondi . Dzina lakuti “ njoka yakale ija ” limatikumbutsa zimene zinacitika mu Edeni pamene Satana ananyenga Hava mwa kugwilitsila nchito njoka . Ulemu ndi ulemelelo zili pamaso pake . Mphamvu ndi kukongola zili m’nyumba yake yopatulika . ” — Salimo 96 : 4 - 6 . 23 N’ndani Akutsogolela Anthu a Mulungu Masiku Ano ? Cingakhalenso bwino ngati angapange ulendo wa ubusa ku banja lanu . Barbara wa ku Canada wa zaka 74 anakamba kuti : “ Ndimayesetsa kuti ndizioneka bwino . Paulo anakambanso kuti Mulungu , “ kucokela mwa munthu mmodzi anapanga mtundu wonse wa anthu , kuti akhale padziko lonse lapansi . Anthu akatinyoza popanda zifukwa zingakhale zovuta kupilila . Masomphenya otsatila a Zekariya aonetsa kuti zimenezi zidzacitikadi . ( Chiv . 21 : 14 ) Conco , panalibe cifukwa cosankhila munthu wina kuti aloŵe m’malo mtumwi wokhulupilika aliyense amene anatsiliza utumiki wake wa padziko lapansi . Inuyo simunaloŵemo , ndipo ofuna kuloŵamo munawatsekeleza ! ” Pokhala Mboni za Yehova , dzina la Mulungu n’lofunika kwambili pa kulambila kwathu . 7 : 21 , 22 ) Yuda anafotokoza za anthu amene adzafooka mpaka kufika pokhala opanda “ mzimu wa Mulungu . ” — Yuda 18 , 19 . ( b ) N’ciani cionetsa kuti Mulungu wathu amakonda anthu a zinenelo zonse ? Takamba conco cifukwa cakuti Baibo imene inali kugwilitsidwa nchito m’machechi panthawiyo ( yochedwa Vulgate ) inali ya Cilatini . Mulungu amafuna kuti mukhale na umoyo wacimwemwe mwa kucitanso zinthu zina zofunika kuposa zimene nyama zimacita . Mateyu 11 : 28 - 30 Kodi nkhani imeneyi itiphunzitsa kuti sitiyenela kumwa zakumwa zina zoledzeletsa tisanapite ku misonkhano yacikristu ? Atapanga ophunzila atsopano kumeneko , io molimba mtima anabwelelanso ku Lusitara ngakhale kuti kucita zimenezo kunali koopsa kwambili . Olo zinali conco , mwadala Adamu anasankha kukana Atate wake wacikondi wakumwamba na kugwilizana ndi mngelo wosamudziŵayo potsutsa cifunilo ca Mulungu . Mau a Mulungu amaonetsa kuti ufulu wathu uli na polekezela , ndipo sitiyenela kulumpha malile amene Yehova anatiikila . 3 : 19 . Kodi Sebina anali ndani ? Nanga ni khalidwe liti loipa limene iye anayamba kukhala nalo ? Anthu aconco , Yehova amawakonda kwambili . ( b ) Nanga Baibo imatiphunzitsa ciani za ufulu umenewo ? Ndipo tikambilana mafunso ati ? KODI MUNGAYANKHE BWANJI ? ( Sal . 18 : 35 ) Conco , timatsatila malangizo ouzilidwa akuti : “ Valani cifundo cacikulu , kukoma mtima , kudzicepetsa , kufatsa , ndi kuleza mtima . ” ( Akol . Citani zimenezo olo kuti izi zingaphatikizepo makambilano a usiku kwambili . muli ndi Mau a Mulungu olembedwa mwa njila yosavuta kumva ? Munthu aliyense amafuna ciani ? Conco , ndinakhala paubale wapadela ndi Atate wanga wakumwamba , ndi onse amene ‘ amafuula kuti : “ Abba , Atate ! ” ’ Mzimu woyela wa Yehova wamphamvuwo unawalimbikitsa ndi kuwathandiza kupitiliza kucitila umboni . ( Salimo 83 : 18 ) Conco , timalambila Yehova Mulungu yekha ndipo monga Mboni zake , timauzako ena za dzina lake . — Yesaya 43 : 10 - 12 . 12 - 14 . ( a ) N’ciani cimene ena amacita akapatsiwa cilango na Mulungu ? Tisaleke kusonkhana pamodzi , monga mmene ena acizolowezi cosafika pamisonkhano akucitila . Zimenezi zinali zovuta kwambili , cakuti nthawi zina ndinali kulakalaka kubwelela kwathu . Baibulo limacha Yesu kuti “ Mwana wobadwa yekha wa Mulungu ” cifukwa analengedwa mwacindunji ndi Yehova . — Yohane 3 : 18 ; Akolose 1 : 13 - 15 . Munthu amene amakhululuka amamvetsa mfundo yakuti tonse timalakwa , kapena kucimwa , m’mau na m’zocita . ( Miy . 15 : 22 ) Izi ziphatikizapo kukambitsilana za thandizo la mankhwala limene makolo angafune . ( Chivumbulutso 11 : 18 ) Ena amafuna kudziŵa ngati tikukhala m’nyengo imeneyo . Mwacitsanzo , onani nkhani zakuti “ Baibulo Limasintha Anthu ” mu Nsanja ya Mlonda yogaŵila . Ronald Curzan N’cifukwa Ciani Anavutika Ndi Kufa ? Anthu onse okhulupilika adzakhala angwilo . Mwana wake wacitsikana anamwalila . Dzina la Mulungu lili ndi tanthauzo lalikulu kwa anthu a Mulungu , ndiye cifukwa cake a m’Komiti Yomasulila Baibulo la Dziko Latsopano analemba dzina la Mulungu m’Baibuloli . 130 : 6 . 5 : 11 , 12 . ( Ŵelengani Yoswa 21 : 45 ; 23 : 14 . ) ( Ower . 11 : 36 , 37 ) Iye analolela kukhala wosakwatiwa na wopanda ana , ndipo analibenso mwayi wosunga dzina la banja lawo kapena wolandila coloŵa . Zonsezi ndi ciyambi ca masautso . ” — Mateyu 24 : 6 - 8 . M’dzikoli , makhalidwe oipa ali ponse - ponse . Koma cifukwa codalila Mulungu amene “ ali pafupi ndi anthu a mtima wosweka , ” timapilila . Nthawi zina n’nali kukwela boti poyenda ku zisumbu zina . Kuyambila nthawi imeneyo , otsalila amene adzalamulila pamodzi ndi Yesu kumwamba , ndiponso a “ khamu lalikulu ” amene adzapulumuka mapeto a dzikoli ndi kulowa m’dziko latsopano , akhala akusonkhanitsidwa . Ngati cimeneci sindiye colinga , mphatso yaconco ingabweletse mikangano na mavuto ena . Anaonjezela kuti : “ Laciŵili lofanana nalo ndi ili , ‘ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ’ ” — Mat . Zimenezi zinacitika zaka zambili Yeremiya atanena mau amenewa . Mfumu Herodi inalamula kuti ana onse aamuna a ku Betelehemu a zaka ziŵili kapena kucepelapo aphedwe . TSAMBA 17 • NYIMBO : 88 , 24 ( Mat . 25 : 14 - 18 ) Pa cifukwa cimeneci , ena angafunse kuti , ‘ Ngati Yesu sanawapatse matalente , kodi afunikiladi kulalikila ? ’ ( Gen . 1 : 31 ) Komabe Satana anamupandukila ndipo kucokela nthawi imeneyo , ndi anthu ocepa cabe amene akucita cifunilo ca Mulungu padziko lapansi . Pamene tinayamba utumiki wa umishonale mu 1979 , magazini ya Nsanja ya Olonda anali kufalitsidwa m’zinenelo 82 cabe . A Yohane : Ndinacita maphunzilo okhudza cikhalidwe ca anthu ndi mbili yakale . Kodi mumaika misonkhano , ulaliki , ndi phunzilo laumwini pamalo oyamba pa umoyo wanu ? Kapena mumakonda kwambili zosangulutsa ? Mau ake abwino analimbikitsa anthu amene mophiphilitsa anali ngati bango lophwanyika kapena monga nyale yofuka imene yatsala pang’ono kuzima . ( Mat . KODI mukukumana na mavuto , monga matenda , umphawi , kapena cizunzo ? Na imwe angakuthandizeni cimodzi - modzi . Ngakhale simukumuona panopa , mumakhulupilila mwa iye . ” — 1 PET . Mafunso amenewa ndi amene Sidnei wazaka 24 , wa ku Brazil amadzifunsa . Koma kodi zimenezi n’zotheka ? M’nthawi ya atumwi , aneneli onyenga ndi anthu ampatuko anali kale pa nchito yofooketsa mpingo wacikristu . Aliyense amene analandilako alendowo na kuwapatsa malo ogona , anapatsiwa kalata yomuyamikila . Pamene mpandawo unali kupelekedwa kwa Mulungu , nyimbo zoimbiwa mwapadela zinacititsa kuti pa mwambowo pakhale cisangalalo cacikulu . Conco , mu April 1949 , ine na amayi tinagulitsa katundu wathu amene tinali naye m’nyumba ya lendi , ndipo wina tinapatsa anthu ena . Ngati timadziyang’ana mosamalitsa pagalasi imene ndi Mau a Mulungu ndi kuona zolakwika zina , monga kudzikonda , tingafooke . 6 : 3 . M’mau ena tingakambe kuti munthu wotelo amakhumudwa cifukwa ca kusakhutila na ndalama zimene ali nazo . Iye anatambasula dzanja lake n’kukhudza wakhateyo , ndipo mwacikondi anati : “ Ndikufuna . Cifukwa colema , nthawi zambili n’nali kulova kusukulu . Zoonadi , kulimbikitsa ena kunali cinthu cofunika kwambili kwa Paulo . Zili conco , cifukwa mphepo na mafunde a m’nyanja zingacititse kuti sitimayo iyambe kuyenda njila yolakwika . Bwanji ngati mkazi wanu si Mboni , ndipo muona kuti sakulemekezani ? Tingatsatile motani citsanzo ca Asa ? Tsiku lina ndinafuna kulasa munthu ndi mfuti , koma mpholopolo inagunda kansimbi ka palamba wake ndi kugwa pansi . ( Maliko 4 : 10 ; 9 : 35 - 37 ) Ngakhale n’conco , ophunzila amenewo sanali ndi njala ya kuuzimu . Izi zimanithandiza kuti nisamangoganizila zinthu zokhumudwitsa zimene angacite , koma kuti niziganizila za mmene ningamuthandizile . ” Cifukwa cakuti tinakhulupilila Yehova ndi Yesu , ndipo tinakhulupililanso kuti adzatithandiza . — Yohane 14 : 1 ; ŵelengani 1 Petulo 2 : 21 . Mbadwa zimenezi zidzapatikizapo anthu ambili amene anafa . Fotokozani zimene tingacite kuti tiziimba mwamphamvu na mokweza . M’nthawi ya atumwi , Ufumu wa Roma unali pamtendele . Katherine atalalikila kwa zaka zingapo m’gawo limenelo , anaganiza zosamukila ku dela kumene anthu angamvetsele uthenga wa Ufumu . Iye anati , “ Ndisanasamuke ndinali kuŵelenga nkhani za anthu amene anali kuyewa kunyumba mu Nsanja ya Mlonda . Musalole kuti zinthu zosafunika zikusokonezeni kutumikila Yehova ( Onani ndime 7 ) mu Nsanja ya Olonda ya December 1 , 2014 . Ili pa intaneti pa www.jw.org . Kodi nthawi zina mumaona kuti n’zovuta kukhalabe wacimwemwe potumikila Yehova ? Nkhani zapoyela zimenezo , zimene masiku ano timati Msonkhano wa Anthu Onse , zinapeleka mipata yabwino yophunzitsa anthu coonadi ca m’Malemba . Iye anachula Febe kuti “ mlongo wathu , ” ndipo analimbikitsa abale kuti ‘ amulandile mwa Ambuye mmene analandilila oyelawo , ndi kumuthandiza pa nkhani iliyonse imene angafune thandizo lawo . ’ Yehova sasintha colinga cake , conco sadzasintha zimene amayembekezela olambila ake kucita . Banja ni mgwilizano wamphamvu kuposa mgwilizano uliwonse umene munthu angakhale nawo . Ndipo cikondi ndiye cingateteze banja kuti lisaipitsidwe , popewa kukhala “ thupi limodzi ” na munthu amene si mwamuna kapena mkazi wake . M’bale George Gangas anati , “ Msonkhanowu unanicititsa kukhala na colinga cakuti nisadzaphonye msonkhano uliwonse . ” Tingapewe kugonjela ku zilakolako zathu ngati nthawi zonse tikhala chelu kuzindikila macenjezo alionse , ndi kucitapo kanthu mwamsanga kuti tiongolele . Mu 1966 n’natulutsidwa m’ndende ndipo tonse anayi tinakukila kumzinda wa Armavir , pafupi na Nyanja Yakuda . Mabuku a Cigiriki amenewo anayamba kuchedwa kuti Septuagint ya Cigiriki . Mungasankhe kuculuka kwa zimene mufuna kuphunzila . N’kuthekanso kuti Yuda anaphunzila za Inoki kucokela kwa Yesu . Yesu anali kuona zocita za Inoki cifukwa cakuti pamene Inoki anali na moyo pa dziko lapansi , Yesuyo anali kumwamba . ( Sal . 119 : 176 ) Tikapeza munthu wina amene anafoka ndipo anasiya kusonkhana , tizimupatsa malangizo acikondi ndi othandiza kuti abwelelenso m’gulu la Mulungu . Cofunika kwambili ni mtendele komanso mgwilizano m’cikwati . ” — Ethan . Popeza kuti alibe mphamvu zokwanila za kuzindikila , zimawavuta kusiyanitsa coyenela na cosayenela . ( Aheb . Mafumu aciyuda onse aŵiliwa anacita zoyenela pamaso pa Yehova , koma Asa anatelo ndi mtima wathunthu . Kodi mfundo za Yehova zinganenedwe mwacidule m’mbali ziŵili ziti ? Ayuda ena a mumpingo , kuphatikizapo Baranaba , nawonso anagwilizana ndi Petulo . 21 : 17 - 25 . Komabe sitiyenela kum’konda mwamwambo cabe . Mau amene Davide anakamba poyankha Goliyati ndi olimbikitsa ngakhale masiku ano . Olo n’conco , m’maiko osiyana - siyana , ambili amadzipeleka kugwilako nchito zomanga malo olambilila . Titafika ku America , tinayamba kukhala kumadzulo kwa mzinda wa Colorado kumene makolo anga anali kukhala . Izi ndi zimene Paulo anacita . 2 : 13 - 16 . Angelo okhulupilika amacita cidwi na umoyo wa anthu , ndipo ni odzipeleka kucita cifunilo ca Yehova . 1 : 7 ) Conco , akulu - akulu a mzinda wa Filipi ayenela kuti anayamba kucita mantha kuzunza Akhristu a mumpingo umene unakhazikitsidwa mumzinda wawo . 21 Tiziyamikila Kukoma Mtima Kwakukulu Kumene Tinalandila Pambuyo pakuti Aisiraeli akuthupi apanduka , Yehova sanafune kuti akhale wopanda anthu omuimila padziko lapansi . Motelo , m’nthawi ya atumwi , iye anasankha Isiraeli wa kuuzimu kukhala anthu ake . Monga a m’banja la cikhulupililo , timafuna kuthandizana kucita bwino mbali zathu m’banja kapena mumpingo . Sitili na maganizo ongofuna mpando ndi kuchuka , ngati mmene anthu amacitila kunjaku . — 1 Tim . Angakuthandizeni kukhala na ‘ cilakolako ’ cophunzila Mau ake . Mlongo wina amakhala kutali ndi makolo ake pamtunda woyenda maola anai pa galimoto . Imfa nayonso , monga mdani womalizila , idzaonongedwa . ” Fanizo loyamba ndi lokhudza akapolo amene anapatsidwa matalente , ndipo lina ndi lokhudza mmene anthu adzalekanitsidwila monga nkhosa ndi mbuzi . Zoonadi , kwa ise anthu , nyenyezi n’zosaŵelengeka . Kodi n’zinthu ziti zimene anacita kuti afike pobatizika ? Kodi nidzakwanitsa kusamalila banja langa ? — 1 Ates . Cinali covuta kuzoloŵela cikhalidwe ndi umoyo watsopano . Koma cifukwa cakuti n’nali wosakwatila , sizinanivute kuzoloŵela . ” Kunyumba imeneyi , kunali kukhala anthu ambili monga okalamba ndi ena obwela kudzaphunzila . Yesu anakamba kuti “ nzelu imatsimikizilika kuti ndi yolungama cifukwa ca nchito zake . ” M’nkhani ino , n’zosatheka kukambilana za akazi onse okhulupilika ochulidwa m’Baibulo . Cifunilo ca Mulungu n’cakuti “ anthu kaya akhale a mtundu wotani apulumuke , ” cifukwa dipo ‘ likucotsa ucimo wa dziko . ’ — 1 Tim . Mukapanga keke kapena masikono , mufotokozeleni nchito ya lesipi . ( Ŵelengani Afilipi 2 : 5 - 8 . ) Baibulo limatilangiza momveka bwino kuti : Khalani mwamuna kapena mkazi wabwino ndipo muzitsatila miyezo yapamwamba ya Mulungu yokhudza ukwati . Kodi inu mumathaŵila kwa Yehova ? Ndithudi , kuvala bwino ndi kudzikonza moyenelela kumalemekeza Mulungu , amene ‘ amadziveka ulemu ndi ulemelelo . ’ — Sal . ( Yakobo 1 : 17 ) Timayamikila kwambili kuti Yehova amatipatsa zonse zimene tifunikila kuti tikhale ndi moyo komanso osangalala . Bill anayembekezela zaka 30 kuti apeze mlongo womuyenelela . Yasmine nayenso anaona kuti nkhawa zinam’kulila kwambili . Ngati tisinkha - sinkha Mau a Mulungu na kupemphela , tidzalimbikitsidwa kutsatila malangizo a m’Baibo . Ndipo koposa zonse , tingaonetse bwanji cikhulupililo ? ( Luka 4 : 42 - 44 ) Yesu anali kuyenda mitunda yaitali kukalalikila uthenga wabwino , ndi kuphunzitsa anthu ambili mmene angathele . Iye anali wangwilo . Masana a tsiku la msonkhano wapadela umenewo ndinagaŵila buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu limeneli . ” Ena a iwo anagwila nawo nchito yolalikila kwa zaka zambili , ndipo mosapeneka , iye anali kudziŵa zofooka zawo . Koma anakamba zinthu zabwino zimene iwo anacita . Kodi zosankha zathu zingasonyeze bwanji kuti timatumikila Yehova yekha ? Kucita zimenezi kunali kovuta , koma Yehova anandipatsa mphamvu . Iye analemba kuti : “ Ngakhale kuti ndine msilikali wa pamadzi , nikukolola zipatso ndi kutamanda Yehova . ” Ubatizo ( Chivumbulutso 6 : 5 , 6 ) Komabe , pamene abale athu akukumana ndi mavuto ambili , m’pamene timakhala ndi mipata yambili yoonetsela kuti timawakonda . Kodi Yehova anaika makonzedwe anji otithandiza kukonzanso ubwenzi wathu na iye ngati tacita chimo ? Komanso Khoti Lalikulu la Ayuda likanaona kuti Akhiristu akupandukila cipembedzo ca Ayuda . ( b ) N’cifukwa ciani makolo onse aŵili amafunika kulelela ana ao pamodzi ? Kukamba zoona , ngati tipitiliza kuganizila zinthu zimenezi , mpata ukapezeka tingazicite . Pindulani na Zimene Mumaŵelenga m’Baibo , Na . Iwo anali kudziŵa kuti sitingathawe . Ponipatsa moni , nthawi zonse amamwetulila na kunikumbatila . ( Mat . 18 : 10 ) Iye anali kutanthauza kuti angelo amacita cidwi na wophunzila aliyense , osati kuti munthu aliyense ali na mngelo womuteteza . — wp17.5 , peji 5 . Asayansi amakhulupilila kuti mu mlalang’amba wathu cabe , wochedwa Milky Way , muli nyenyezi zokwana 400 biliyoni . Mwamuna wake atamusiya , Sabina anali kuvutika kupeza zofunikila mu umoyo wake ndi ana ake acitsikana aŵili . 12 : 17 - 19 ; 41 : 14 , 39 - 41 ; Eks . 1 : 22 – 2 : 10 ) Cifukwa cokhulupilila Yehova , “ Wosaonekayo , ” Mose molimba mtima anapita kwa Farao kukamuuza mau onse amene Yehova ananena . Cina cimene cingawalimbikitse kucita izi , ni kukumbukila kuti kumvela ni lamulo locokela kwa Mulungu , Atate wa ife tonse . Nanga n’cifukwa ciani linalembedwa ? MWAUKALI , wapolisi wina ananiuza kuti : “ Iwe ndiwe tate woipa kwambili . Satana anatsutsa kuti Yehova ndi woyenela kulamulila pamene anapandukila Mulungu . Idzafotokozanso zimene tingacite kuti tipewe kubwelelanso ku umunthu wakale . Pamene Adamu anaona Hava kwa nthawi yoyamba , iye anasangalala kwambili cakuti sanabise mmene anali kumvelela pamene ananena ndakatulo yake . Akazi ena amamva monga mmene Rosa anadandaulila kuti : “ Ndinali monga wanchito wa amuna anga . ” Ngakhale kuti Danieli anapatsiwa cakudya ca mfumu , “ anatsimikiza mumtima mwake kuti sadzidetsa . ” ( Dan . Mukamaliŵelenga , limakubwezani kumbuyo kudziko lakale limene lingaoneke ngati lacilendo kwa inu . Tidzasangalala kwambili Yehova akadzayankha pempho limeneli mwa kucotsapo Satana ndi kuononga dziko lake . Timawagaŵilanso zofalitsa zofotokoza Baibulo . Palinso zolengedwa zina zauzimu zimene zinakhala zoipa ndipo zinagwilizana ndi Satana . Kutsogolo : Alyona , Raya , na Svetlana 14 : 12 ) Pogogomezela kufulumila kwa nchito imeneyi , Yesu anati : “ Tiyenela kugwila nchito za iye amene anandituma ine kudakali masana . Usiku ukubwela pamene munthu sangathe kugwila nchito . ” — Yoh . 9 : 4 . Ngati makolo saonetsa cikondi cacibadwa kwa ana awo , cingakhale covuta kuti anawo aziwamvela na mtima wonse . Masiku ano , kuyenda kumawavuta cifukwa ca kuŵaŵa mendo . M’dziko la Kanani munagwa njala yaikulu . Leka cabe zimene umacita kuti utulutsidwe . ” Kuti mudziŵe zimene munthu amalakalaka muyenela kukhala mmvetseli wabwino . M’pempheni kuti akupatseni nzelu kuti muzisamalila bwino thanzi lanu . Ananitumiza ku ndende ya pa cisumbu ca Yíaros ( Gyaros ) , cimene cili pamtunda wa makilomita pafupi - fupi 50 kum’maŵa kwa cisumbu ca Makrónisos . Nimaona kuti n’nasankha mwanzelu kwambili pamene ninayenda kukatumikila kosoŵa . ” Ndi zitsanzo ziti zoonetsa nkhani zina zokhudza ulosi zimene zili m’Baibulo ? 11 : 7 ; Miy . 29 : 25 ) Kukhala ndi Ciyembekezo ceniceni kumatithandiza kupilila mayeselo ndi kuyembekeza za mtsogolo molimba mtima . ( Sal . Cifukwa cakuti amatikonda , tili ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo kwamuyaya m’Paladaiso pano pa dziko lapansi . Nanga mau a pa Deuteronomo 6 : 4 , 5 amatikhudza bwanji masiku ano ? Anafotokozanso cifukwa cake maganizo a dziko angakhale okopa kwa anthu opanda ungwilo . Kodi manje tiyenela kucita ciani ? — Vesi 34 . Cimatithandizanso kukhalabe oyela mwakuuzimu , mwamakhalidwe , mwamaganizo ndi mwakuthupi . Kutumikila Yehova kumabweletsa cimwemwe coculuka . Kapena lembani m’ndandanda wa maina a anthu amene mufuna kudzalankhula nao akadzaukitsidwa . Kodi Baibo ingakuthandizeni pa mavuto aakulu ngati amenewa ? Pamene Yesu anali pa kacisi , anaona zimene mkazi wamasiye wosauka anacita . ( Yakobo 3 : 2 ) Kuti tithetse kusamvana , tiyenela kucita zimene tingathe kuti ‘ tifunefune mtendele ndi kuusunga . ’ Kodi gawo lake n’lotani ? Ophunzila oyambilila anali kuyenda m’njila zabwino zimene Aroma anapanga . Koma nsapato zophiphilitsa zimene Akhristu amavala , zimawathandiza polalikila uthenga wa mtendele . ( Yes . 2 : 24 , 25 ; 3 : 9 , 10 ) Conco , io anakhala anthu ‘ oomboledwa ’ ndi Yehova . — Eks . 15 : 13 ; ŵelengani Deuteronomo 15 : 15 . Polalikila , tidziwafotokozela anthu kuti Ufumu wa Khiristu ukayamba kulamulila pa dziko lapansi , anthu adzasangalala ndi zinthu zabwino cifukwa ca dipo , ndipo adzayamba kukhala angwilo pang’ono - pang’ono . Ndine woyamikila kwambili kuti Yehova ananikokela kwa iye ndi kwa olambila ake , amene ananiphunzitsa moleza mtima ndi mokoma mtima kugwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo pa umoyo wanga . Ndi maganizo otani amene tiyenela kupewa ? Kodi masinthidwe amenewa akhudza bwanji zofalitsa zathu ? Cipembedzo coona cimatiphunzitsa kulemekeza mnzathu wa m’cikwati , kuona malumbilo a cikwati kukhala opatulika , kupewa ciwelewele , kuphunzitsa ana kukhala aulemu , ndi kukhala na cikondi ceni - ceni . 24 : 15 ) Zimenezi si maloto ai . Ngati tiika Mulungu patsogolo , iye ‘ adzatidalitsa . ’ — Yelekezelani ndi Genesis 39 : 3 . Nkhani yotsatila iyankha mafunso amenewa . Tisanayankhe funso limeneli , tifunika kumvetsetsa zimene Baibo imakamba ponena za anthu auzimu , kapena kuti okonda zauzimu . Pa tsiku lothela la msonkhanowo , m’bale wina anaika ndalama m’thumba la jekete ya Riana . M’FANIZO la matalente , Yesu anafotokoza momveka bwino za udindo umene otsatila ake odzozedwa ali nao . Anapililanso mavuto na kusintha kwa zinthu mu umoyo wake . Mwamunayo akumvetsela mwachelu kwa M’bale Russell , mkambi wa imvi ndi ndevu zambili , amene wavala jekete yaitali yakuda . “ Aliyense wochula dzina la Yehova aleke kucita zosalungama . ” — 2 TIM . Kucita zimenezi kudzatithandiza kupilila zinthu zofooketsa ndi kukhala citsanzo cabwino . — Aroma 12 : 20 , 21 ; Akolose 3 : 13 . 2 : 7 - 9 ; 1 Tim . Ukapolo umenewu unayamba pambuyo pa caka ca 100 C.E . , kufikila pamene kacisi wauzimu wa Mulungu anayeletsedwa m’nthawi ya mapeto . — Machitidwe 20 : 29 , 30 ; 2 Atesalonika 2 : 3 , 6 ; 1 Yohane 2 : 18 , 19 . Si kulakwa kuti Akhristu azisangalala poceza ndi acibale kapena anzawo pa Intaneti . Buku la Chivumbulutso limatitsimikizila kuti Satana wangotsala ndi “ kanthawi kocepa . ” Kusinkha - sinkha zimene mwaŵelenga N’namvela monga kuti mtolo wolema wacoka pa mapewa anga . ( Maliko 8 : 38 ) Ngati cosankha cathu cacititsa kuti pakhale kusamvana pakati pa ise na abululu athu amene si Mboni , tingacite ciani kuti ticepetse mikangano na kukhalabe okhulupilika ? Tiyeni tikambilane zimene tingacite . Lipezekanso pa webusaiti ya jw.org kapena mungaunike QR khodi iyi . Iwo amasankha kukhala ndi umoyo wosalila zambili , ndi kugwila nchito imene dzikoli limaona kuti ndi yotsika kwambili . Amacita zimenezi kuti akwanitse kutumikila Yehova mmene angathele . ( 1 Tim . Koma Afarisi anali opanda cifundo . Iye anati : “ Nikakumana ndi anthu aukali , nimayesetsa kukumbukila lemba la Miyambo 19 : 11 , imene imati : ‘ Kuzindikila kumacititsa munthu kubweza mkwiyo wake . ’ M’busa wabwino amadziŵa kuti nkhosa ina ingacoke pagulu ndi kusoŵa . 10 , 11 . ( a ) N’cifukwa ciani n’zosavuta kuyamba kukonda kwambili zinthu za m’dziko ? Ndi phindu lokhalitsa liti limene tidzapeza tikakhalabe ogwilizana ? ( b ) Nanga Mau a Mulungu anakhudza bwanji atsogoleli a anthu a Mulungu ? Ndiyeno , mozizwitsa anacititsa Petulo kugwila nsomba zambili , ndipo anamuuza kuti : “ Kuyambila lelo uzisodza anthu amoyo . ” ( Aroma 5 : 1 , 2 ) Umenewu ni mwayi wa mtengo wapatali . Tiyeni tione zimene Baibulo limaphunzitsa . Anawauza malipilo amene adzawapatsa ndipo anthuwo anavomela . Unali ulendo wautali ndithu mwina wa masiku 4 kapena 5 kuyenda pansi . Patatsala milungu iŵili kuti akakambe nkhani yake yoyamba , ndinamufunsa ngati anali kuyeseza . Kodi munthu aliyense , cinthu ciliconse , ndi cocitika ciliconse m’fanizoli , cimaimila cinacake codzacitika mtsogolo ? ( Mateyu 6 : 9 , 10 ) Tikuyembekezela mwacidwi kudzaona pemphelo limeneli likuyankhidwa , pamene Ufumu wa Mulungu udzabweletsa madalitso ambili kwa anthu . Iye anasangalala kwambili kuwaona akubwela ali bwinobwino kucoka ku nkhondo . 29 : 22 ) Onani mmene ofalitsa ena aŵili a Ufumu anasinthila khalidwe lawo lokonda kukwiya , na kuyamba kukhala mwamtendele ndi anthu ena . Cikhulupililo cidzatithandiza kuona cithunzi m’maganizo mwathu ca mmene umoyo udzakhalila mu Ufumu wa Mulungu . Timadziŵa mmene Mlengi wathu alili , timakhudzika mtima ndi cikondi ndi cilungamo cake , ndipo timam’sanzila . — Ŵelengani Mlaliki 12 : 13 ; Mika 6 : 8 . Umunthu watsopano umene umalengedwa “ mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu ndipo umatsatila zofunika pa cilungamo ceniceni ndi pa kukhulupilika , ” ungathandize okwatilana kupewa ciwelewele . Makolo anga ananibatiza ku Chalichi ca Katolika , ndipo m’kupita kwa nthawi ndinaloŵa m’gulu la oyimba khwaya . 8 : 5 , 40 ; 21 : 8 ) Paulo ndi ena anapita kukatumikila kumadela akutali . ( Mac . Zimene n’nali kucita pa umoyo wanga zinali zosiyana kwambili ndi mfundo za makhalidwe abwino za m’Baibulo . Acicepele angaphunzile maluso amene angafunikile akadzakula . Tingathandizenso abale na alongo amene asamukila m’dela lina m’dziko lawo kapena amene asamukila m’dziko lina , kukatumikila kumene kuli olengeza Ufumu ocepa . Kucita izi kudzakuthandizani kudziŵa mmene mungaseŵenzetsele mfundo za m’Baibo mu umoyo wanu . Odzozedwa okhulupilika ndi “ oyenelela Ufumu wa Mulungu . ” Mwacitsanzo , sitolo yaikulu ya ku Seoul imene tachula m’nkhani yapita ija inagwa cifukwa cakuti akuluakulu a boma analola omanga sitoloyo kugwilitsila nchito zipangizo zosalimba ndi kuphwanya malamulo a kamangidwe kovomelezeka . ( Sal . 37 : 10 , 11 ) Ndife otsimikiza kuti Yehova sadzacedwa ngakhale ndi tsiku limodzi , kuwononga dziko loipali . — Hab . Koma ena angafike pozoloŵela kwambili kucita zinthu zimenezi . Sin’nali wokonzeka . ” Kapolo wokhulupilika ndi wanzelu waonetsa cikhulupililo capadela mwa kuchukitsa ndi kufalitsa uthenga wabwino wa Ufumu mwakhama . Tingadziŵe bwanji mmene Yehova amaonela zinthu ? “ Mukhale otsanzila anthu amene mwa cikhulupililo ndi kuleza mtima akulandila zinthu zimene Mulungu analonjeza monga colowa cao . ” — AHEBERI 6 : 12 . Gidiyoni anadabwa kuti pamene mngelo anaonekela kwa iye anamucha kuti “ munthu wolimba mtima ndi wamphamvu . ” Abale oyendela oimilako bungwe lolamulila , anali kufikitsa kumipingo “ malamulo oyenela kuwatsatila , malinga ndi zimene atumwi ndi akulu ku Yerusalemu anagamula . ” Ndi masautso otani amene tinganene kuti ndi acindunji ? Nimakondwela ngako kudziŵa kuti lomba ku Armavir kuli mipingo 6 , ndipo ku Kurganinsk kuli mipingo inayi . Ai ndithu , Baibulo limatiuza kuti : “ Munthu akakhala pa mayeselo asamanene kuti : “ Mulungu akundiyesa . ” Uwu ndiwo umoyo wokondweletsa kopambana . ” Pamene Yefita anafika kucoka ku nkhondo , munthu woyamba amene anamulandila anali mwana wake wamkazi wokondedwa . 2 : 44 ) Anthu ambili amaganiza kuti Mulungu sadzaononga dongosolo loipali , koma Baibulo limanena zosiyana kwambili ndi zimenezi . ( Zef . Ngati n’conco , ni makhalidwe ati amene adzakuthandizani kukhala monga dothi lofewa limene Yehova angaumbe ? Zimene ndinali kuphunzila ku chalichi , sizinandithandize . Kodi ‘ tingalimbikile ’ bwanji kutsatila lamulo langwilo ? MARITA , amene anali wophunzila wa Yesu komanso bwenzi lake anali na cisoni . Kodi amakhudza umoyo wanu ? Tsopano ndili ndi umoyo wokhutilitsa . ” Mwa kupatsa anthu zinthu pa kampeni kapena kucita zinthu zina zake , olemela anganyengelele anthu kuti asankhe munthu amene io akufuna . YESU anakambilatu kuti m’masiku otsiliza uthenga wabwino wa Ufumu udzalalikidwa kwa anthu onse . Ngamila imodzi ikakhala ndi ludzu kwambili , ingamwe madzi okwana malita 95 . N’zoona kuti si zonse za m’dzikoli zomwe ndi zoipa . Mwacitsanzo , ndimakondwela kuphunzitsa anthu kuti adziŵe mmene nsembe ya dipo ya Kristu imagwilila nchito , ndi mmene idzatithandizila kukhala ndi moyo wosatha m’dziko la mtendele ndi lolungama . ” Kodi iye anapeleka mwana wake ku cihema kuti akatumikile Yehova kwa moyo wake wonse ? M’bale Sergio anati : “ Kwa kanthawi ndithu , sitinali kupita pa malo athu ocitila ulaliki wa poyela cifukwa codwala . Nayenso Yosefe , mdzukulutubzi wa Abulahamu , anaonetsa khalidwe la kuleza mtima . Ndiyeno anaudandaulila kuti : “ Yerusalemu , Yerusalemu , wakupha aneneli iwe ndi woponya miyala anthu otumizidwa kwa iwe . 16 : 7 ) Monga atumiki a Mulungu , sitifunika kungovala ciliconse cimene takonda . Kodi yacokela pa webusaiti imene aliyense amalembapo maganizo ake , kapena yacokela pa webusaiti yosadziŵika bwino ? Pofotokoza vuto lake kwa mkaidi mnzake , kodi Yosefe anakamba mwamphwayi ngati kuti safuna kutuluka m’ndendemo ? Kudziŵa cifukwa cimeneco kungatithandize kuona kuti moyo uli ndi colinga . Kodi tiyenela kuyopa kuti Mdyelekezi na ziŵanda zake adzamvetsela zimene tikamba m’pemphelo na kuzigwilitsila nchito polimbana nase ? Sicinali copepuka kuti Inoki alengeze uthenga waciweluzo umenewo kwa anthu onse amene anafunika kuumva . ( a ) Kodi Timoteyo anaphunzila bwanji cikhristu ? Nanga anacita bwanji na zimene anaphunzilazo ? Komanso cifukwa ca kusamvela kwao , anthu onse anali pa njila yopita ku imfa . Lembani fomu ya pa Intaneti yofunsila phunzilo la Baibulo pa www.jw.org . Tinakondwela kwambili ndi makhalidwe a Mboni za Yehova monga cikondi , mgwilizano ndiponso kudzipeleka kwao pothandiza ena . — Yohane 13 : 34 , 35 . Mwacitsanzo , analembela mpingo wa ku Kolose za Akhristu onama amene anali kuyesa kukondweletsa Mulungu mwa kutsatila Cilamulo m’malo mokhulupilila Khristu . ( Akol . Komabe , Paulo anali kulembela amene anali “ ku Roma monga okondedwa a Mulungu , oitanidwa kukhala oyela . ” 12 : 8 ) Nthawi zina m’Malemba cofufumitsa cimaimila coipitsa kapena ucimo . N’ciani cingaticititse kufunsa funso lakuti : “ Mpaka liti ? ” Pamenepo , pali mafunso monga akuti : “ Mukamapemphela , kodi mumachula mwacindunji zimene mukufuna ? Coonadi cokamba za Yehova Mulungu cinayamba kuzika mizu m’dziko la Kyrgyzstan ca m’ma 1950 . Mwacitsanzo , ponena za “ Gogi wa kudziko la Magogi , ” Baibulo limati : “ Iwe udzabwela m’dzikolo ngati mphepo yamkuntho . m’magazini ino . Koma panthawiyi , n’nali kufunitsitsa kukhala ndi mtendele wa m’maganizo umene Baibulo imakamba . Kuonjezela apo , iye amawapempha kukhala osiyana ndi dzikoli limene ladzaza ndi makhalidwe oipa . Kudzicepetsa kungatithandize bwanji kupewa kudalila nzelu zathu ? ( Sal . 147 : 15 - 18 ) Inde , Mulungu wathu wanzelu zopanda malile ndi wamphamvuyonse , amene amalamulila “ cipale cofewa ” ndi “ madzi oundana ” kapena kuti matalala , angatithandize kupilila mavuto aliwonse amene tingakumane nawo . ( 1 Akor . 10 : 6 , 7 , 11 , 12 ) Monga mmene Paulo anakambila , ngakhale olambila oona angayambe makhalidwe ena oipa . Bwenzi labwino limakambilana ndi mnzake mokoma mtima ndi momasuka . N’ciani cam’thandiza kudziŵa zimenezo ? Lupanga ndi uta zimaimila njila imene Kristu adzagwilitsila nchito kuononga adani ake . Zimenezi zitanthauza kuti Myuda ameneyu si munthu mmodzi koma akuimila gulu lonse la odzozedwa . Wofalitsayo afunika kupatsidwa malangizo acindunji kucokela kwa mphunzitsi wokoma mtima ndi wacikondi . Koma koposa zonse , analola mzimu wa Yehova kumutsogolela . Koma mwina inu mungafunse kuti : Kodi Baibulo limanena nthawi pamene mapeto adzafika ? Pokweza ucifumu wake , n’cifukwa ciani tinganene kuti Mulungu adzaonetsetsa kuti wakwanilitsa malonjezo ake ? Conco , abale anali kuyamikila nikawathandiza kuwongolela mmene anali kucitila misonkhano na ulaliki . Kodi Luka anakamba kuti n’ciani cinacitika kwa Utiko ? Nanga izi zinawakhudza bwanji anthu ena ? Anthu amene amadya zizindikilo za pa Cikumbutso amatsimikiza ndi mtima wonse kuti ali m’pangano latsopano . Muyenela kudalila Yehova molimba mtima ndi kukhala wosasunthika pocita zinthu zimene muona kuti ndiye zoyenela ndi zanzelu . Koma kodi n’ciani maka - maka cimene cinawacititsa cidwi ? Buku ina inati : “ Palibe buku ina yakale zungulile dziko lonse imene mau ake ali na maumboni ambili monga Cipangano Catsopano . ” — The Books and the Parchments . Anthu ambili padziko lonse amalemekeza kwambili Baibulo . Joel , wa zaka 21 , amene akhala ku Guam , anati : “ Akulu amaonetsa kuti amandidalila mwa kundipatsa zocita pa mpingo . ( Luka 2 : 1 - 5 ) Nthawi ina , pamene Paulo anaimbidwa mlandu , anadzichinjiliza mwaulemu ndi kupeleka ulemu woyenelela kwa Mfumu Herode Agiripa ndi Fesito , bwanamkubwa waciroma woyang’anila cigawo ca Yudeya . — Mac . 37 : 11 ; Yes . Cikhulupililo ndi limodzi mwa makhalidwe amene mzimu woyela umatulutsa . Cigumula cisanacitike , Lameki mbadwa ya Seti , anali kulambila Yehova . ( Yakobo 1 : 19 ) Mariya anali mmvetseli wabwino . 23 Kodi Mumacita Zinthu Mogwilizana ndi Cilungamo ca Yehova ? Iye anali kufika pa misonkhano ya mpingo , koma sanali kufuna kuphunzila Baibulo . Yesani kudziŵa mayeselo amene amakumana nawo omwe angafooketse cikhulupililo cawo . Ndipo athandizeni mmene angacitile nawo . Ndinali kukonda Mulungu , koma sindinasangalale ndi zimene anali kuphunzitsa ku machalichiko . Atazindikila kulakwa kwake , analapa , ndi kubwelela kwa makolo ake . Angafunikenso kujaila zinthu monga kupeleka misonkho , kulipila mabilu , kupita kusukulu yatsopano , kucita zinthu panthawi yake , ndi kulangiza ana . Yehova anawatsimikizila kuti adzawapatsa mtendele ndi kuwateteza kuti agwile bwino nchito yawo yomanga . Iwo anali oyamba pa anthu amene anayamba kulengeza mbili yabwino , ndipo anali mbali ya kukwanilitsidwa kwa ulosi wa Yesu wakuti : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” — Mat . A Zimba : Iyai , sindikumbukila . Ponena za mmene tingapezele zinthu zofunika paumoyo , Yesu anati : “ Siyani kuvutika mumtima ; . . . Atate wanu amadziŵa kuti zinthu zonsezi n’zofunika kwa inu . ” — Luka 12 : 29 - 31 . Zofalitsa zonse zimene timalandila monga mabuku , mabulosha , ndi magazini zimacokela kwa Yehova . Cikomyunizimu na cikhulupililo cakuti kulibe Mulungu zinali zozika mizu mwa ine kwa zaka 18 . Pafupi - fupi caka cimodzi m’mbuyomo , M’bale James A . Komanso cifukwa cokonda abale athu , tidzapewa kuwakhumudwitsa . Mfundo zomveka bwino zimenezi za m’Cilamulo cimene Mulungu anapatsa Aisiraeli zaka mazana zapitazo , zingagwilebe nchito masiku ano ku makhoti . Kodi Mose analosela ciani ? Nanga mau ake anakwanilitsidwa motani ? Filipo anauza anthu Acigiriki uthenga wolimbikitsa umenewu . — Yohane 12 : 20 - 26 . Pocita zinthu ndi anthu amene mumakonda komanso anzanu , kodi mungatengele kukhulupilika kwa Sara ? Kodi akuimila ciani pamodzi na okwelapo ake ? Makolo anga sanapiteko , koma ine n’napita . Mwina inu mwadzionela nokha kuti , “ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” ( Mac . ( Luka 10 : 27 ) Nchito ni njila cabe yotithandiza kukwanilitsa udindo wathu . ▪ Samalani ndi Anthu Ogwilizana Nao Masiku Ano Otsiliza Ndiyeno , Mulungu anagoneka Adamu tulo tofa nato , anam’cotsa nthiti imodzi , ndipo ‘ anapanga mkazi kucokela kunthiti ” imeneyo . Nowa atafa , Mulungu anapitilizabe kutsogolela anthu ake . M’nkhani ziŵilizi , tidzakambilana mafunso amenewa na ena . Munthu amafunika kusankha mmene adzagwilitsila nchito moyo wake . ” Iye ataona kuti wakwanitsa kukhala , anabwelela kwao ku Japan kuti akakonzekele zodzakhalilatu m’dzikoli . Sitikudziŵa cifukwa cimene mayiyo anacitila zimenezo cifukwa sanali wacibale wathu . Nthawiyo inali kuchedwa Mtendele wa Aroma . Panthawiyo , boma la Roma linaletselatu kuukila boma kulikonse . Koma anali kufuna kuti ulemelelo wonse uzipita kwa Atate wake . Conco mukamaona zizindikilozo , mumatsimikiza mtima kuti mwakhala pang’ono kufika . Mu 1979 , modzifunila ndinayamba kulemba m’ndandanda wa mau a Cituvalu ndi matanthauzo ake . Olo kuti n’nali kukhala kutali na mkazi wanga ndi ana anga , n’nalimbikitsidwa kudziŵa kuti ine na Maria takhalabe wokhulupilika kwa Yehova . Omvetselawo akuomba m’manja poonetsa kuti akuvomeleza zimene m’baleyo wakamba . Kuti cikwati cikhale colimba , aŵiliwo afunika kukhala ololelana pa kupanda ungwilo kwawo . Yesu anali kudziŵa nthawi yoyenela kukhala cete ndi nthawi yoyenela kulankhula . 12 , 13 . ( a ) Ngati mwana wacotsedwa , kodi makolo acikhristu angaonetse bwanji kuti amamvela Mulungu ? Conco , timapemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele . 3 : 12 ) Olungama amaphatikizapo “ khamu lalikulu ” limene ‘ lidzatuluka m’cisautso cacikulu . ’ M’baleyo anapitiliza kukamba kuti : “ Sanali kunilola kukamba nkhani . . . Iwo anali atalalikila ngakhale kuti anatsutsidwa ndi anthu komanso ziwanda . Cimene ndimayamikila kwambili n’cakuti ngakhale kuti amandikonda , iye amakondanso Yehova koposa . idzathandiza bwanji kuti colinga ca Mulungu cikwanilitsike ? Panthawiyi ndinali ndi ana atatu , apo n’kuti ndili ndi zaka 24 . Ganizilani mmene Mulungu anacitilapo kanthu pofuna kukoka anthu oyenelela . Khala woyela . ( Miy . 2 : 2 , 3 ) Comaliza , zimene taphunzila tiyenela kuzigwilitsila nchito paumoyo wathu . Monga mmene ulosi unanenela , mtendele ‘ unacotsedwa padziko lapansi ’ ngakhale kuti mayiko akhala akucita mapangano a mtendele . ( Yobu 42 : 3 - 6 ) Nthawi zina , nafenso tingalephele kuona dzanja la Mulungu cifukwa ca mavuto amene tikukumana nao . Muzifunafuna mipata yolalikila mwamwai . Kuti tikhale aphunzitsi abwino , tifunika kumacita zimene timaphunzitsa . Ena anali kuganiza kuti : ‘ Popeza fano ni cinthu copanda pake , munthu angadye nyamayo ndi cikumbumtima coyela . ’ Tifunika kuwapanga kukhala mabwenzi athu ndi kuwathandiza kuona kuti ni ofunika mumpingo . ( 1 Akor . Asanadzipeleke kwa Mulungu , iye anali na vuto lopeza zifukwa anthu ena , ndiponso anali kukamba mokhadzula kwa makolo komanso abale ake . Timafuna kuthandiza anthu kukhulupilila kuti Yehova Mulungu ndi munthu weniweni amene io angamuyandikile . Malinga ndi Cilamulo ca Mose , matenda a mkazi ameneyo anam’cititsa kukhala wodetsedwa , ndipo aliyense womukhudza anali kuonedwa kukhala wodetsedwa . — Levitiko 15 : 19 , 25 . Kodi ndimaona coonadi kukhala camtengo wapatali mofanana ndi io ? Nditaphunzila Baibulo kwa caka cimodzi , ndinadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa , potengela citsanzo ca mkazi wanga . 6 : 7 ) Cinanso cimene cingakuthandizeni ni kuzindikila kuti nthawi zina mumafunikila malangizo ocokela kwa ena . Buku la Levitiko n’lothandiza kwambili pa nkhani ya ciyelo . Koma anthu anawalenga kuti azikhala padziko lapansi . Pamene timulambila sitimupangitsa kukhala wolemela , kapena wamphamvu kwambili . ( 2 Akorinto 1 : 3 , 4 ) Mwacitsanzo , panthawi ina pamene Yesu anapanikizika maganizo , “ anagwada ndi kuyamba kupemphela . ” Anthu 36 anapezeka pamsonkhano umenewu , ndipo anthu 8 anabatizika . Sukuluyi inali kutali kwambili na kwathu cakuti amayi na ambuya sanali kukwanitsa kukaniona . Komanso , anzanga ena ananithandiza pamene ine ndi ana anga tinali kukukila ku nyumba ina . Mwacionekele , zimenezo zinakukondweletsani . Kodi tili na zonse zofunikila zimene zingatithandize kupanga zosankha zokondweletsa Yehova ? Mwana wa Abulahamu , Isaki , nayenso anakhala ndi cisoni kwa nthawi yaitali . Kodi Sukulu ya Gileadi yathandiza bwanji ? ( Luka 4 : 43 ) Tikupemphani kuti mukambilane ndi Mboni za Yehova m’dela lanu kapena pitani pa Webusaiti yathu ya jw.org . Yesaya 33 : 24 : “ Palibe munthu wokhala m’dzikolo amene adzanene kuti : ‘ Ndikudwala . ’ ” Hachi yakuda , imene wokwelapo wake ali ndi sikelo m’dzanja lake imene ikuimila njala . Ndi malemba ati amene angathandize m’bale kusintha maganizo ake ngati safuna kukalamila udindo ? ( Genesis 24 : 62 ) Rabeka ayenela kuti anaona nkhosa . Iye sanacite zimenezo kuti atikhumudwitse . Arabi Achiyuda anali kuphunzitsa kuti akazi safunika kuceza ndi amuna amene si acibale ao , ngakhale kuyenda nao pamodzi . N’zoona kuti sitingawapeweletu anthu a makhalidwe oipa . Ganizilaninso Aroma 6 : 19 imene imati : “ Pelekaninso ziwalo zanu kuti zikhale akapolo a cilungamo kuti muzicita nchito za ciyelo . ” 1 : 24 . Komanso , ngakhale maboma amene amaoneka ngati abwino , sangakwanitse kuthetsa mavuto onse a anthu . Ana afunika kumvela makolo awo ndi kuleledwa m’malangizo a Yehova . ( Aef . Posankha njila zopimila matenda kapena cithandizo ca mankhwala , tiyenela kukhala ‘ oganiza bwino ’ ndi osamala . Pamene Yehova anabweletsa Cigumula padziko lapansi , iye anaonetsa mphamvu zake pa anthu opandukawo ndi angelo oipa . 2 : 16 ) Mtumwi Paulo anacenjeza Akhristu anzake za kuopsa kokhutilitsa cilakolako ca thupi . Iye anati : “ Kuika maganizo pa zinthu za thupi kumabweletsa imfa . . . cifukwa kuika maganizo pa zinthu za thupi ndiko udani ndi Mulungu . ” ( Aroma . Stephanie anati : “ N’nafufuza ndi kuŵelenga nkhani zokhudza kutumikila ku malo osoŵa mu Nsanja ya Mlonda . Mwacitsanzo , cifukwa ca tsankho boma ya dziko lina mu Africa inali kuletsa Mboni za Yehova kumanga Nyumba za Ufumu . ( Eks . 3 : 11 ) Koma Yehova anamuthandiza , ndipo m’kupita kwa nthawi , analimba mtima ndi kugwila nchitoyo . Pamwamba pa mapili padzakhala tiligu woculuka . ” Fotokozani . ( b ) Kodi kunyada n’kutani ? Nanga ndi zitsanzo ziti za m’Malemba zimene zionetsa kuti kunyada n’koipa ? 1 : 17 . Tidzakambilananso mmene pemphelo lingatetezele ubale wathu ndi Yehova , mosasamala kanthu za mmene zinthu zili paumoyo wathu . Koma Eliya anawalimbikitsa kuti asankhe kulambila Yehova , Mulungu woona . Mungathandize bwanji ana anu acinyamata ngati mumavomeleza zolakwa zanu ndi kupepesa ? Nanga n’ciani cimene tingacite kuti tikhale odziletsa kwambili ? ( Chivumbulutso 12 : 17 ) Conco , ambili mwa Akristu a 144,000 anafa kale ndipo ali kumwamba . Malinga n’kunena kwa buku ina , iye anaseŵenzetsa liu la Cigiriki limene limatanthauza “ kucitila wina zabwino mwa cisomo cako , mosayembekezela cobwezela ciliconse . ” Tifunikanso kukumbukila kuti nsembe ya dipo la Khristu , imationetsa cikondi cacikulu cimene Yehova na Yesu anatisonyeza . Yehova anatikonda popeleka Mwana wake monga nsembe yotiombola , ndipo Yesu nayenso anatikonda polola kutifela . Conco ndinali kucita kuti ndikaona anthu aŵili akumenyana , inenso ndinali kugwapo . NJILA YOTHETSELA VUTOLI : Mu Ufumu wa Mulungu simudzakhala kampeni kapena masankho cifukwa cakuti ufumuwu udzalamulila kosatha . N’cifukwa ciani tifunika kupewa kucita zimenezi ? 6 : 13 . Tingacitenso bwino kuganizila madalitso amene Yehova wasungila anthu onse amene amayandikila kwa iye . — Yak . ( Yohane 10 : 16 ) Iwo amakhala ndi miting’i mlungu uliwonse m’makomiti amene akutumikila . Tingaphunzile ciani pa citsanzo ca Yesu ? Mungacite ciani kuti cikondi cizikusonkhezelani kuceleza ena ? Kuonjezela pamenepo , angatanthauzenso madalitso a kumwamba amene ali “ m’paladaiso wa Mulungu . ” — Chiv . Iye nthawi zina anali kudzimva monga munthu wovutika . Deut . M’pomveka kuti Yesu anagwilitsila nchito mau akuti “ manda acikumbutso ” cifukwa Yehova adzaukitsa ao amene iye akukumbukila . 32 : 1 , 2 . Muzimvela Yehova . Ndinayamba kugulitsa mankhwala osokoneza bongo ndipo sindinali kusiya mipeni ndi mfuti kulikonse kumene ndinali kupita . Kodi anthu angapindule bwanji na cisomo ca Mulungu ? PACIKUTO : M’bale akucititsa msonkhano wokonzekela ulaliki m’tauni yaing’ono m’dela la St . Tingagwilitsile nchito m’ndandanda wa ziyeneletso za akulu kuti tithandize ophunzila Baibulo athu ndi anthu ena a cidwi kudziŵa mmene akulu Acikristu amasiyanilana ndi atsogoleli a zipembedzo zina . Kodi akulu amatsatila bwanji citsanzo ca Samueli ? Nanga io amamva bwanji akatelo ? Ndipo tidzadalila kwambili ndi kulemekeza abale amene aikidwa pa udindo mumpingo wacikristu . — Aheb . Kodi Mulungu Wamphamvuyonse waonetsa bwanji kuti amatha kulamulila mphamvu za cilengedwe ? Ena atumikila panthambi za kumaiko akwao kwa zaka zambili . Kodi si zoona kuti ngati anthu m’dziko ndi a ziphuphu , boma limene angapange nalonso limakhala la ziphuphu ? Kodi kudziŵa Mulungu molondola kunam’thandiza bwanji Danieli ? Masomphenya a Ezekieli asonyeza kuti anthu a Mulungu anakhalanso ndi moyo , ndiponso anamasulidwa ku cipembedzo conama pang’onopang’ono . Kodi anakonzekela bwanji ubatizo ? Ngakhalenso mmene Yehova anakhululukila Aisiraeli pamene analapa cigololo cawo cauzimu . ( Hos . Mosiyana ndi zimenezi , Baibulo limakamba kuti pemphelo limaposa mankhwala . Cinyengo : Ndi kunamiza munthu wina kapena kum’pusitsa pofuna kum’dyela masuku pamutu , kapena kupezelapo mwai wina wake Mofananamo , tikalakwitsa , kaya sitinacitile dala kapena ena sanazindikile , kodi sitiyenela kuvomeleza kuti talakwa ? Mneneli Ezekieli ndi Zefaniya anakambilatu kuti golide na siliva , zinthu zimene amalonda amaziona kukhala zofunika ngako , zidzakhala zopanda phindu . ( Ezek . 1 : 5 , 23 . Tidziŵa bwanji kuti lemba la Salimo 118 : 22 linalosela za kuuka kwa Yesu ? Musamayembekezele kucita zinthu mwangwilo , koma vomelezani kuti monga munthu aliyense , na imwe mudzalakwitsa zinthu zina . — Mlaliki 7 : 20 Patapita zaka zoposa 1,000 , kucokela pamene salimoyi inalembewa ndiponso patapita mawiki angapo pambuyo pakuti Yesu wamwalila na kuukitsidwa , Petulo anakamba na khamu la Ayuda ndi anthu otembenukila ku ciyuda za mau a pa Salimo 16 : 10 . Paul anaonanso kuti cinthu cofunika kwambili cimene aliyense angacite , ndi kukhulupilila Mulungu . Pokhala Akhiristu odzozedwa , mamemba a kapolo ameneyo “ amatsatila Mwanawankhosa kulikonse kumene akupita . ” ( Chiv . Patapita nthawi , ndinayamba kuona kuti chalichi mofanana ndi anthu ena onse , cinali kulephela kuthandiza anthu ovutika . Komabe , panatenga nthawi kuti nisinthe . Ndinaleka kukhulupilila “ oyela mtima ” komanso moto wa helo ndipo sindinali kuona kuti wansembe angakhululukile macimo . Koma anthu a Yehova sanapheko munthu aliyense . Mwacionekele , tsiku la ubatizo linali lofunika kwambili ndi losangalatsa pa umoyo wanu . Posakhalitsa , ndinamva monga cinacake caphulika m’thupi mwanga . Pangani Malemba kukhala maziko a nkhani yanu . ( Yoh . Kodi atumiki ena okhulupilika a Mulungu amavutika ndi ciani ? Uziseŵenzetsa luso lako la kulingalila kuti ‘ uzindikile tanthauzo ’ la zimene uŵelenga . Buku limeneli limafotokoza zimene tingaphunzile kwa io , osati ponena za zimene nkhanizo zimaimila . Mu 607 B.C.E . , Ababulo anagonjetsa ufumu wakumwela wa Yuda umene unali ndi mafuko aŵili . Muziika zinthu zofunika kwambili patsogolo , muziona zinthu zotheka , muzipatula nthawi yopumula tsiku lililonse , muzisangalala na cilengedwe ca Yehova , muzikhala wansangala , muzicita masewela olimbitsa thupi kawili - kawili , ndi kugona mokwanila . — w16.12 , mapeji 22 - 23 . Yesu atatsala pang’ono kugwidwa ndi kuphedwa , anapempha Atate wake kuti : “ Abba , Atate , zinthu zonse n’zotheka kwa inu . Ndicotseleni kapu iyi . 3 , 4 . ( a ) Fotokozani cifukwa cake sitiyenela kuonetsa Khalidwe Lopambana kwa Akristu anzathu okha . ( b ) Kodi tikambilana ciani m’nkhani ino ? Akuluakulu a boma ndiponso anthu a m’dziko nthawi zambili amacita zinthu mwadyela ndi modzikonda . 24 : 3 - 8 ; Luka 21 : 10 , 11 ) Pali maumboni ambili amene aonetsa kuti Ambuye Yesu Kristu “ anapatsidwa cisoti cacifumu ” m’caka ca 1914 . Tingatengele bwanji cikhulupililo ndi kumvela kwa Danieli ? ( b ) Kodi Alexandre anapindula bwanji ndi thandizo la mkulu wina ? Nthawi zonse , tiyeni tizisonyeza kuti timayamikila mphatso imeneyi . Mwacitsanzo , angamulande bolayo na kum’bisila kwa masiku angapo . N’tafika zaka 14 , n’nali kufuna kuyamba upainiya . Cikondi ndi kuopa Mulungu zinan’thandiza kuti nisinthe . ” Cikhulupililo cathu cimalimba tikaganizila mmene Yesu anakhalila wolimba mtima pamavuto . Tiyenela kukhala ndi colinga cokhazikitsa mtendele ndi abale athu Anali kucita zimenezi n’colinga cakuti asunge mapangano ao . Kodi Yesu anacita ciani mogwilizana ndi tanthauzo la dzina lake ? N’cifukwa ciani sitiyenela kukhumudwa tikaona kuti cikhulupililo cathu cayamba kufooka ? ( Danieli 2 : 44 ) Monga tanenela kale pa mfundo yacitatu , amene adzaonongedwa ndi “ mafumu a dziko lapansi , ndi magulu ao ankhondo , ” amene adzasonkhana kuti “ amenyane ndi wokwela pahatchi uja ndi gulu lake lankhondo . ” — Chivumbulutso 19 : 19 . Mu June 1940 , n’taima pakhomo n’naona mathilaki onyamula asilikali ambili akudutsa . Yehova analamula anthu ake kuti aseŵenzetse mkuwa pomanga cihema . Pambuyo pake , anawalamulanso kuseŵenzetsa mkuwa pomanga kacisi ku Yerusalemu . ( Eks . Cifukwa malamulo onena kuti , ‘ Usacite cigololo , usaphe munthu , usabe , usasilile mwansanje , ’ ndiponso lamulo lina lililonse limene lilipo , cidule cake cili m’mau awa akuti , ‘ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ’ imatiteteza ? Citsanzo canu n’cofunikanso kwambili pothandiza ana anu kukhulupilila zimene amaphunzila . Kodi zinthu zidzakhala bwanji cionongeko citapita ? Zotulukapo zake , tidzakhala na cifuno couzako ena zimene timakhulupilila . — Ŵelengani Salimo 73 : 28 . Mwezi wa Nisani utafika , Yesu anapita ku Yerusalemu kukacita Pasika potsatila malamulo a Atate ake . Tiyelekeze kuti m’bale akuganizila mmene angapitile patsogolo mumpingo . Toñi analalikila mzimayiyo ndi kuyamba kuphunzila naye Baibo . Zonsezi n’cifukwa ca khalidwe lake la kufatsa ndi la mtendele . N’zomveka kuti mwacibadwa timakonda malo athu , cikhalidwe ndi cinenelo cathu , kapenanso zakudya za m’dziko limene tinakulila . Ngakhale kuti maboma ambili masiku ano amatilola kusatenga mbali m’ndale , tiyenela kuyembekezela kuti adzatikakamiza kutengamo mbali pamene tiyandikila mapeto . Banja lina limene tinali kuphunzila nalo Baibo limakhala kutali kumudzi wina wosauka kwambili . Taphunzilanso kuti Yehova anauzila olemba Baibulo ndi mzimu woyela , ndipo io analemba maganizo ake osati ao . Ndipo Yehova anamugwilitsila nchito kucita zinthu zazikulu . ( 1 Sam . 17 : 33 - 37 , 50 ; 1 Maf . Pamene anamaliza nkhani yake , abale ndi alongo anaomba m’manja mokhudzidwa mtima kwa nthawi yaitali , ndipo ena anagwetsa misozi poona khama la mwana wa sukulu watsopano ameneyu . Kevin , amene ni mkulu mu mpingo , anati : “ Cimene cinatithandiza kwambili ine na mkazi wanga ni kucita upainiya wothandiza titangofika mu mpingo watsopano . Kodi tingaphunzitse bwanji cikumbumtima cathu ? Kodi pa Malaki 3 : 10 pali lonjelo lanji ? Ganizilani zimene zinacitikila Yesu pa nthawi imene anatsala pang’ono kucoka padziko lapansi . N’zomveka kuti Mose anafunsa Yehova kuti : “ Ndine ndani ine kuti ndipite kwa Farao ndi kutulutsa ana a Isiraeli ku Iguputo ? ” Itilimbikitsanso kutengela Yesu mwa kugwilitsila nchito mphatsoyi polemekeza Mulungu ndi kulimbikitsa ena . Kodi Ramiro anasankha kucita ciani kuti akhale ndi cimwemwe pa umoyo wake ? Mboni za Yehova zinandionetsa buku la Chidziŵitso Chotsogolera ku Moyo Wosatha , * limene muli nkhani zimene zinayankha mafunso anga . Kukamba mau oipa okhudza munthu wina kungapangitse kuti vuto likule kwambili ( Onani palagilafu 14 ) Kodi Yehova anaonetsa bwanji kuti anali kum’dziŵa Yesu komanso Mariya ? Mwina anthu amenewo anali anzanu kapena acibale anu . Khalani odzicepetsa , ofikilika , na oyamikila . Mogwilizana ndi fanizo la zofufumitsa , pelekani zitsanzo zoonetsa mmene nchito yolalikila Ufumu yapitila patsogolo . N’ciani cingathandize munthu kuti asinthe ? Tidzaphunzila cifukwa cake tifunika kudzipeleka kwa Mulungu kuti apitilize kutikonda . Iye anakambanso kuti : “ Ukasamukila kudela lina , uyenela kuzindikila kuti kuphunzitsa ena kumacitika m’njila zosiyanasiyana . ” Atandilimbikitsa conco , ndinawapempha kuti azindiphunzitsa Baibulo kaŵili pa mlungu , ndipo ndinayamba kupezeka pa misonkhano yao yacikristu . Pakuti Ziyoni wamva zoŵaŵa za pobeleka ndipo wabeleka ana ake aamuna . ” Komanso bwanji ngati muona kuti akulu anacitila cifundo munthu wolakwa popanda zifukwa zomveka bwino ? Ngati makolo anu amakhala okha , tsimikizilani kuti anthu odalilika amene amawasamalila ali ndi makiyi kuti azitsegula nyumbayo ngati pagwa zamwadzidzidzi . Iye nthawi zonse anali kupita m’masunagoge , kumene Ayuda anali kulambilila Mulungu , ndipo anali kukambilana nao za m’Malemba . — Ŵelengani Machitidwe 17 : 1 , 2 . ( Ŵelengani Salimo 34 : 6 , 18 , 19 ; 1 Petulo 5 : 6 , 7 . ) Yesu anathandiza ophunzila ake kulimbitsa cikhulupililo cao mwa zocita ndi zokamba zake . A Zulu : Cabwino , tiyeni tikambilane . Iye anali munthu wangwilo ndipo anali ndi maluso abwino kwambili kuposa munthu wina aliyense , koma sanali wodzikweza . Kulalikila m’gawo la cinenelo cina kunaticititsa kudzimva monga takhalanso acinyamata . Conco , kuti ticisunge , tifunika kuciseŵenzetsa bwino na kupitiliza kucita zinthu zotithandiza kucikonda kwambili . Ngakhale kuti poyamba ndinali kuvutika kwambili kupita mu ulaliki , ndinayamba kusangalala kwambili ndi ulaliki , cakuti mu 1998 ndinakhala mpainiya wa nthawi zonse . Motelo sanakanakhala ndi mwai wokwatiwa ndi kukhala ndi ana . Yehova amakonda anthu , ndipo afuna kuti anthu omvela akakhale mmene iye anali kufunila . Koma cifukwa cakuti anaganizila zimene anaphunzila ndipo anakhutila nazo . ​ — Ŵelengani Aroma 12 :⁠ 1 . NKHANI YA PACIKUTO — AMUNA ANAYI OKWELA PA MAHOSI — KODI AMAKUKHUDZANI BWANJI ? 31 - 32 . M’kupita kwa nthawi , Yehova anacita cipangano ndi ana a Yakobo ( Isiraeli ) . OLOŴETSEDWAMO : Yesu ndi Isiraeli wa kuuzimu Ndipo zimenezi zidzaonetsa kuti tikusunga mosamala Mau a Mulungu . — Sal . Kumasuka kwa Aisiraeli mu ukapolo ku Iguputo kumaposa kumasuka kulikonse kwa akapolo m’mbili ya anthu . Pambuyo polongosolela a Komiti Yoona za Ntchito Yolemba Mabuku mavuto amene omasulila amakumana nao , Bungwe Lolamulila linavomeleza kuti pakhale pulogalamu yophunzitsa omasulila onse padziko lonse . Motowo unaphanso anthu oposa 1,200 . Posapita nthawi , alonda andende ndi akaidi anayamba kunifunsa cifukwa cimene ninaloŵela m’ndende , ndipo ninali wokondwa kuwafotokozela cikhulupililo canga . ( Luka 21 : 28 ) Ndithudi , panthawiyo sitidzacita mantha , koma tidzakhala ndi cikhulupililo cakuti tipulumuka . Ku Britain , anthu anali kuganiza kuti nkhondoyo idzakhala “ nkhondo yothetsa nkhondo zonse . ” Atate ake a Antoine anali atavulazidwa pamene m’godi unawadilikila , conco banja silikanacitila mwina koma kuuza Antoine kukagwila nchito yakalavulagaga maola 9 pa tsiku . Nkhaniyo imati : “ Cotelo iwo anauzana kuti : ‘ Tamuonani wolota uja . Taona kuti Yehova amakonda kwambili aliyense wa ife ndipo amafunitsitsa kuti zinthu zizitiyendela bwino . ” Munamulonjeza kuti mudzam’konda ndi kum’tumikila ndi mtima wanu wonse kwamuyaya . N’ciani cimene Aisiraeli anayenela kucita ataona umboni woonekelatu wakuti amunawo anali kutsogoleledwa na mzimu woyela ? 1 : 8 ) Koma zimenezi sizicitika kaŵili - kaŵili , ndipo Akhristu okhulupilika sadabwa kapena kukhumudwa akacitilidwa zinthu zopanda cilungamo . Zofalitsa zogaŵila . Mwamunayo anati : “ Conde ndipatse madzi a mumtsuko wako ndimweko pang’ono . ” Akulu akamatumikila modzicepetsa , abale na alongo amawakonda ndi kuwalemekeza ( Onani palagilafu 13 - 15 ) Ndipo tingatengele citsanzo cake mwa kuyesetsa kulalikila kwa aliyense , olo amene aoneka kuti sangalabadile . Mlangizi wathu wina ku Sukulu ya Giliyadi , m’bale Jack Redford , anatiuza kuti poyamba tingadabwe , ngakhale kukhumudwa ndi malo amene tidzatumikilako , maka - maka poona umphawi wa anthu . Kodi khalidwe lalikulu la Mulungu ndi liti ? Satana Mdyelekezi ni wokwiya ngako , ndipo “ akuyendayenda uku ndi uku ngati mkango wobangula , wofunitsitsa kuti umeze winawake . ” ( 1 Pet . Paulo anachulanso kufanana pakati pa mfumu komanso Melekizedeki ndi Yesu . ( Aheb . Pankhaniyi , Baibulo likutikumbutsa kuti palibe cobisika pamaso pa Yehova . Anakambanso kuti iye ndi anthu ake sanali kudziŵa cocita . Mfundo yakuti anayenela kukumana ndi “ masautso ambili ” inaoneka kukhala yokhumudwitsa , osati yolimbikitsa . Kenako , Yesu anayamba kugwila nchito ndi Mulungu , ndipo anali “ pambali pake monga mmisili waluso . ” Pa tsiku limene Yesu anayambitsa Mgonelo wa Ambuye , iye anapemphelela ophunzila ake kuti akhale ogwilizana ngati mmene iye alili wogwilizana ndi Atate wake . Yesu atakamba kuti tifunika kuona Akhristu anzathu monga abale na alongo , anagogomezanso kufunika kokhala odzicepetsa . Nimakondwela kwambili kucita upainiya kuno . Zoonadi , muyenela kuyamikila Yehova m’pemphelo cifukwa ca zinthu zabwino zimene muli nazo . ( 1 Ates . Ofalitsa onse 49 a mu Mpingo wa Feijó , anatengeledwa kukhoti cifukwa cocita msonkhano m’nyumba ya anthu popanda cilolezo . Kukamba zoona , si copepuka kukhala wofatsa m’zocitika ngati zimenezi . Cikalata cothetsela cikwati cimene cinalembedwa mu 71 / 72 C.E . Banja lathu linali kupemphela ku Chalichi ca Maronite , cimodzi mwa machalichi a Akatolika a ku m’maŵa . Zekariya anauziwa kuti akatenge siliva na golide kwa Heledai , Tobiya , ndi Yedaya , amuna atatu amene anali atafika kumene kucokela ku Babulo . Anamuuzanso kuti zinthuzo apangile “ cisoti cacifumu caulemelelo . ” ( Zek . 14 - 16 . ( a ) N’zinthu zina ziti zimene gulu lakhala likucita poseŵenzetsa zopeleka zanu ? Mwasintha zinthu zina ndi zina paumoyo wanu kuti muzithela nthawi yaitali mu ulaliki . Kodi mwapindula bwanji poseŵenzetsa zida zimene tili nazo ? Pasanapite nthawi yaitali , Hagara anakhala ndi pathupi pa Abulahamu . Mvetselani kwa mboni . Ciŵelengelo cimeneci cikuonetsa kuti pa anthu 18 alionse mu Zambia , munthu mmodzi anapezeka pa Cikumbutso . Koma n’nadabwa cifukwa n’nakangiwa kupeleka umboni wakuti kulibe Mulungu . N’ciani cinacititsa banja lina kukhulupilila kuti Yehova anawacitila cifundo ? Mothandizidwa ndi Yehova , tsopano nili na mtendele wa m’maganizo ndipo ndine wodekha , koma kale n’nali monga bomba yoteya - teya . N’nali wamkali ndipo n’nali kukwiya kwambili na zinthu zocepa . ” Cifukwa abale ake anali kumuzonda ndi kum’citila nsanje , anam’thamangitsa m’dzikolo kuti asalandile colowa cake monga mwana woyamba kubadwa . ( Mateyu 24 : 38 , 39 ; 2 Petulo 2 : 4 - 6 ) Molingana ndi masiku akale , masiku ano , Mulungu pamodzi ndi a angelo ake oyela ambili - mbili , ni okonzeka kupeleka ciweluzo kwa anthu osaopa Mulungu . Pa zaka zoculuka zimene iye na mkazi wake anatumikila Yehova , anakumana na zothetsa nzelu zambili . Koma Akhristu ambili panthawiyo anali “ kulengeza uthenga wabwino wonena za Khristu ” mwacangu . Anali kucitanso zinthu zina zoonetsa kukonda Mulungu , kukonda Akhristu anzawo , ndi anthu osakhulupilila . ( Mac . Yezebeli anapanga ciwembu ca kupha ana a Naboti mwina cifukwa coganiza kuti io adzatenga munda wa mpesawo monga colowa cao . N’zimene zingacitikenso kwa imwe . Anthu amene amapanga gulu la okana Kristu amatsutsa Kristu ndi ziphunzitso zake . Filipi linali dela lolamulidwa ndi ufumu wa Roma . ( Aroma 5 : 12 ) Ngakhale ndi conco , banja likhoza kuyenda bwino masiku ano . Ngati kukhala wosakwatila si lamulo , n’cifukwa ciani Yesu ndi Paulo anakambapo za ubwino wokhala mbeta ? Iye anakhazikitsa nthawi zoikidwilatu komanso anaika malile acikhalile a malo oti anthu azikhala . A Zulu : Sindinu nokha a Zimba amene mukulephela kumvetsetsa ulosiwo . Ngakhale mneneli Danieli sanamvetsetse bwinobwino tanthauzo la zimene anauzilidwa kulemba . Pa Yohane 15 : 4 - 10 , Yesu anagogomeza kufunika kwa khalidwe la kupilila mwa kuseŵenzetsa mau angapo otanthauza “ kukhalabe . ” Amatilimbikitsanso kuika maganizo athu pa dziko latsopano limene Mulungu watilonjeza . — Ŵelengani 2 Petulo 3 : 11 - 13 . Magazini tachula ija inatsiliza na mau akuti : “ Mkhrisu amene afuna kudziŵa ngati n’koyenela kuseŵenzetsa tuzipangizo twa IUD , ayenela kupenda mosamala mfundo ngati zimenezi , na kupanga cosankha mogwilizana na zimene Baibo imakamba pa nkhani ya kulemekeza moyo , umene ni wopatulika . ” — Sal . MAULOSI A MULUNGU AMASIYANA NDI A ANTHU Nthawi zambili anthu amalosela zinthu zozikidwa pa kafukufuku wa sayansi , maumboni a zinthu zina , kusintha kwa zinthu , kapena pa mauthenga abodza onenedwa ndi Akristu onama . ( b ) N’ciani cimene munthu amene amadya zizindikilo ayenela kucita akacimwa ? Limenelo si lamulo wamba limene lingacotsedwe kapena kusinthidwa pofuna kusangalatsa ena . Conco , pamene iye anali kukula , anafunika kupanga cosankha . Kunena zoona , kudalila Atate wathu osati cuma ndiye njila yokha yopezela cimwemwe ceniceni ndi kukhala otetezeka . — Ŵelengani Mateyu 6 : 24 , 25 , 31 - 34 . Dziko loipali likadzawonongedwa , n’zinthu ziti zimene inuyo mufuna kudzacita ? TSAMBA 6 • NYIMBO : 86 , 104 Mau ndi zocita zake zimakondweletsa Mulungu . “ Timakumbukila nthawi zonse nchito zanu zacikhulupililo , ndi nchito zanu zacikondi . ” — 1 ATES . Kuphunzila za mbili yakale n’kosangalatsa . Ndi bwino kudziŵanso kuti zinthu zambili zimene Yesu anakamba ndi kucita ali padziko lapansi sizinalembedwe m’ma Uthenga abwino . Farao anasunga lonjezo lake , ndipo patapita nthawi yocepa anaveka Yosefe malaya amtengo wapatali . COLINGA : Kuyala maziko ovomelezeka akuti a 144,000 akhale ana a Mulungu , ndi kuti apange mbali yaciŵili ya “ mbeu ” Nthawi zina , ifenso mofanana ndi Yehosafati tingasoŵe cocita , ngakhale kucita mantha kumene cifukwa ca mavuto amene takumana nawo . ( 2 Akor . Komanso adzakhala osamva za ena , kapena kuti opupuluma ndi ocita zinthu mosasamala . Ndi macenjezo otani okhudza ciwelewele amene Baibulo limapeleka ? Anthu ena aona kuti zimene Michel de Notredame ( Nostradamus ) analemba m’zaka za m’ma 1500 zikukwanilitsidwa masiku ano . Dipo la Yesu ni mphatso imene Yehova anapeleka kwa inu . Davide anazindikila kuti Yehova anaseŵenzetsa mkaziyo , pofuna kum’teteza kuti asacite zinthu zimene zikanam’pangitsa kukhala na mlandu wamagazi pamaso pa Mulungu . Zimenezi zinanithandiza kutenga coonadi kukhala canga , ndipo n’nali kulakalaka kukumana ndi m’busa wina . Ngakhale kuti Paulo na Baranaba anali osiyana zibadwa , iwo anacita utumiki pamodzi asanakangane . Mwacitsanzo tiyeni tiŵelenge pa Danieli 2 : 44 . Adria anati : “ Ngakhale kuti tinali titasintha zinthu zina mu umoyo wathu , tinasinthanso zina ndi zina kuti tikhale ndi umoyo wosalila zambili . ” KODI NDIKUKAMBILANA NDI MUNTHU WOTANI ? tikhala m’dziko loipa ? Loisi ndi mwana wake Yunike , anali atakhala akazi okhulupilika Acikristu , odzala ndi “ cikhulupililo copanda cinyengo , ” cimene Paulo anayamikila kwambili . ( Onani mfundo zina zothandiza m’buku la Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu , mapeji 181 mpaka 184 , kuyambila pa kamutu kakuti “ Kapumidwe Koyenera . ” ) Ayuda ambili amene Yesu anali kuwalalikila anali kufuna kuti azidzilamulila okha osati kulamulidwa na Aroma . Nadine anakamba kuti : “ Kuganizila zosiya ana athu kunali kunidetsa nkhawa . Koma iwo anatiuza kuti : ‘ Mukapita kukatumikila kosoŵa ku dziko lina , tidzakunyadilani . ’ Conco , tidzidziona moyenela ndi kukumbukila kuti ndife opanda ungwilo . Yehoahazi anangolamulila kwa miyezi itatu , kenako anamangidwa ndi Farao wa ku Iguputo , ndipo anafela kumeneko . ( 2 Maf . Nanga n’cifukwa ciani kuphunzila zimenezo n’kothandiza ? Patapita mawiki angapo , n’nayamba kupezeka pa misonkhano , imene inali kucitikila ku cipatala ca M’bale Hardaker . BUKU la Uthenga Wabwino la Mateyu , limati : “ Yesu analoŵa m’kacisi ndi kuthamangitsa onse ogulitsa ndi ogula m’kacisimo , ndipo anagubuduza matebulo a osintha ndalama ndi mabenchi a ogulitsa nkhunda . ( Luka 2 : 38 ; 3 : 15 ) Ambili anali kukhulupilila kuti Mesiya adzakhazikitsa ufumu wake mu Isiraeli . Nkhani ziŵilizi zazikidwa pa malangizo ouzilidwa a Paulo amene analembela Akhristu a ku Kolose . Anadziŵanso kuti Yehova sangakondwele ngati iye wagwilitsila nchito mzimu woyela pofuna kukwanilitsa zofuna zake . Takambilana zitsanzo zabwino ndi zoipa zimene zingatithandize kudziŵa zimene ‘ kuona Mulungu , ’ kapena kuona dzanja la Mulungu kumatanthauza . Alex , amene amagwila nchito pa kampani yonyamula katundu , akuoneka wotopa pamene akunyamula katoni ina ya katundu kuika m’galimoto . Iye anali wosamvela malamulo , anali kugulitsa mankhwala osokoneza ubongo ndiponso anali na mbili yakuti anali wankhanza ngako . Cilango cimakhala cothandiza kwambili ngati cigwilizana ndi zimene mwana walakwa . Yehova walola munthu aliyense kudzisankhila , ndipo walolanso mitu ya mabanja kusankhila mabanja ao . 6 : 19 , 20 . Mwina iye akungofunika kuphunzitsa bwino cikumbumtima cake , kapena cikumbumtima cake cili bwino . Polimbana ndi Basa , n’ciani cinacititsa Asa kudzidalila komanso kudalila anthu ena monga Beni - hadadi m’malo modalila Yehova ? Kodi iwo amakonda kuganizila ciani ? Kuti ticite zimenezo , tifunika kupewelatu macimo akulu - akulu amene anthu ena a ku Korinto anali kucita . Nchito yapadela imeneyi inawalimbikitsa kwambili abale a m’dzikolo . Aroma caputa 8 ili na malangizo amene angakuthandizeni kuti mukapezekemo . Citsanzo ca Rabeka n’colimbikitsa kwambili masiku ano . Kenako adzaona Mwana wa munthu akubwela mumtambo ndi mphamvu ndi ulemelelo waukulu . ” — Luka 21 : 26 , 27 . Inde , mkazi anapha Sisera , m’silikali wankhondo wamphamvu . N’cifukwa ciani n’cosavuta munthu kuyamba kucilikiza mwakacetecete anthu andale omenyela ufulu wodzilamulila ? Kumbukilani cocitika cimene takambilana kuciyambi kwa nkhani ino . 2 : 35 , 45 ) Kucokela pamene Yesu anayamba kulamulila mu 1914 , mapili onse aŵiliwa akhalapo , ndipo athandiza kwambili pa kukwanilitsa cifunilo ca Mulungu pano padziko lapansi . “ Anayamba kuwatanthauzila zinthu zokhudza iyeyo m’Malemba onse , kuyambila ndi Zolemba za Mose ndi za aneneli zonse . ” Adamu atafunsidwa cifukwa cimene iye anapandukila anapeleka cifukwa cosamveka , amvekele : “ Mkazi amene munandipatsayu ndi amene wandipatsa cipatso ca mtengowo , ndipo ine ndadya . ” Njila yacinayi imene tingalimbitsile mgwilizano ni kukonda anthu ena potengela Yehova , amene ni Mulungu wacikondi . Koma aneneli a Yehova anali kungolemba zoona basi , ngakhale zolakwa za anthu a mtundu wawo , ngakhalenso za mafumu awo . Komabe mosiyana ndi Aroni , anthu onsewo anali odzikhudza , ndipo anali kufuna kulanda udindo wa Mose . ( Num . Ndinakhudzidwanso kudziŵa kuti Mulungu ali ndi dzina . M’kupita kwa nthawi , nayenso anatumikilapo m’Bungwe Lolamulila . Kodi ana acikulile ali ndi udindo wotani kwa makolo ao okalamba ? Muzigwila nchito mwa cikati - kati . Nthawi zina , anthu a Yehova anali kucita zopeleka zothandizila anthu amene anali kutsogolela pa nchito yake . Mu 2002 cikhulupililo canga mwa Mulungu cinathelatu . ( Miy . 22 : 3 ) Komanso , muziganizila mavuto amene mungakumane nawo cifukwa cogwilizana ndi anthu ocita zoipa . ( Agal . Ife ndife amene timacita nchito imene Yesu analosela . Pokonzekela Cikumbutso , mungacite bwino kupanga pulogilamu yapadela yoŵelenga imene ingakuthandizeni kuyandikila kwambili Yehova na Yesu . ( b ) N’cifukwa ciani tiyenela kupezeka pa mwambo wokumbukila imfa ya Yesu ? Madzi a m’nyanja imeneyi anayamba kuoneka monga akucepa . 12 , 13 . ( a ) N’ciani cidzacitika pamene Yesu adzabwela “ ndi mphamvu ndi ulemelelo waukulu ” ? ( b ) Kodi Yehova amatithandiza bwanji kukhalabe maso ndi oganiza bwino ? Kuyamika “ Ndi bwino kuyamika inu Yehova . ” — Salimo 92 : 1 . Kodi tiyenela kucita ciani ngati winawake wakamba kapena wacita zinthu zimene zatikhumudwitsa ? Ngakhale nyumba zazing’ono zinali na zitseko zokhala ndi loko . Ndithudi , Yehova amatikonzela phwando la kuuzimu . — Yes . Ndipo zinthu zimene anaphunzila panthawi ya mavuto zinawathandiza panthawi imene Yehova anawapatsa maudindo aakulu . Kuti iwo adziteteze , amadalila mankhwala ocita kuvala , zithumwa , na zinthu zina zamatsenga . Bishopu wina wa ku Germany analemba kuti : “ Iwo ayeneladi kunena kuti cipembedzo cao cokha n’cimene cinakanitsitsa kumenya nao nkhondo mu ulamulilo wa Hitler . ” Yankho limene ambili anapeleka ndi lakuti acinyamata ena pamene anali ana sanali kulimbikitsidwa kukhala ndi zolinga za kuuzimu . SI COCITIKA CODZIDZIMUTSA . ( Yak . 1 : 22 ) ( b ) Ndi zosankha zotani zimene Yehova amadalitsa ? Onani mmene anthu amene akumanapo na mavuto osiyana - siyana apezela citonthozo ceni - ceni kwa Mulungu . Nanga tiyenela kuwamvetsa bwanji mau a Paulo akuti : “ Mulungu . . . sadzalola kuti muyesedwe kufika pamene simungapilile ” ? Koma pali zina zimene mungacite kuti mukhale wolengeza Ufumu wacangu . Conco , m’nthawi ya Yeremiya ndiponso m’nthawi ya Yesu , mau akuti Rakele analilila ana ake anali oyenelela ponena za cisoni cimene amai aciyuda anamva cifukwa ca kuphedwa kwa ana ao . Mogwilizana ndi ulosi wa m’Baibo , anthu ambili masiku ano ni “ okonda zosangalatsa . ” Mmodzi wa iwo “ anabwelela , akutamanda Mulungu mokweza mau . ” Nkhani izi zidzatithandiza kumvetsa kufunika kwa ulamulilo wa Yehova ndi kudziŵa mmene tingaucilikizile . Kodi amamvela bwanji akaganizila zimene anasankha ? Masiku ano , Akhristu amene ndi mitu ya mabanja amadziŵa kuti ali na udindo wa m’Malemba wopezela mabanja awo zinthu zofunika pa umoyo . ( 1 Tim . Poyamba , mau a pa Ezara 4 : 8 - 6 : 18 , 7 : 12 - 26 ; Yeremiya 10 : 11 , ndi pa Danieli 2 : 4b - 7 : 28 analembedwa m’Ciaramu . Kusintha ngati kumeneku ni umboni wakuti cikondi cimene Akhristu ali naco pakati pawo cimagonjetsa tsankho komanso cimatigwilizanitsa mwamphamvu kwambili . — Akol . N’cifukwa Ciani Tifunika Kuphunzila Baibulo ? Mkulu wina amene wathandiza anthu ambili othaŵa kwawo anati : “ Tikangofikila anthu othaŵa kwawo , tifunika kuwauzilatu kuti ndise Mboni za Yehova ndi kuti colinga cathu cacikulu ndi kuwathandiza mwauzimu osati mwakuthupi . Ndiyeno , ŵelengani Salimo 124 : 8 , limene limati : “ Thandizo lathu lili m’dzina la Yehova , Wopanga kumwamba ndi dziko lapansi . ” Fotokozani mmene tingagwilitsile nchito Chivumbulutso 14 : 6 , 7 pokambilana ndi anthu okonda zacipembedzo . Komanso anatenga akazi ena apambali 300 . ( 1 Maf . Mtumwi Paulo anaticenjeza kuti dzikoli likupita pamodzi ndi cilakolako cake . ( 1 Akor . 4 : 6 ) Kambili , tikayamba kucita zinthu mwanjila imeneyi , ndiye kuti mzimu wa kudzikuza wayamba kutiloŵelela . Abale amenewa saona udindo wawo monga mwayi wodzipezela malo abwino okhalapo na mabanja awo . M’malomwake , ambili mwa iwo amakhala pa malo ena alionse , ngakhale amene si abwino kweni - kweni m’cigawo cimene apatsidwa kuti ayang’anile . Yesu anaukitsidwa kuti akhale “ mwala wofunika kwambili wapakona ” ( Onani palagilafu 8 , 9 ) ( Maliko 2 : 15 ) N’zomvetsa cisoni kuti Afarisi sanaone zabwino zimene Yesu anaona mwa anthuwo . Idzafotokoza cimene mkate ndi vinyo zimene timagwilitsila nchito pa Cikumbutso zimaimila . Yesu anakambilatu kuti cizindikilo ca m’masiku otsiliza sicidzakhala mtendele na citetezo koma mavuto . Mfumu Qin Shi Huang anafuna kuti akatswili asayansi apeze mankhwala amene angacititse kuti iye asafe . Ni funso liti limene tiyenela kudzifunsa ? Kumbukilani kuti Timoteyo ‘ anakhulupilila pambuyo pokhutila ’ na zimene anaphunzila . “ Ndimakondwela ndi kucita cifunilo canu , inu Mulungu wanga . ” ​ — SALIMO 40 :⁠ 8 . Yehova Wandidalitsa ( C . ( b ) N’cifukwa ciani Mau a Mulungu amaletsa kugonana na munthu amene suli naye m’cikwati ? Baibulo limafotokozanso cinthu cina comvetsa cisoni cimene cinacitika pamene anthu anali kutsuka galeta la mfumu . Mlongosi wake , Lazaro , anali atamwalila . ( Luka 10 : 5 , 6 ) Tikakhala ndi mzimu waubwenzi polalikila , tingapangitse anthu kukopeka ndi coonadi . Kodi mudzacita zinthu momuganizila ? Pamene akatswili a zacipembedzo anaitana Lefèvre kuti akafotokoze cifukwa cimene analembela zimenezo , iye anangokhala “ cete ” n’kuthaŵila ku Strasbourg . Cinanso , n’nakambilana na makolo anga pa nkhani ya zolinga zanga zauzimu . Kuonjezela apo , analimbikitsa Solomo kuti : “ Tsopano mwana wanga , Yehova akhale nawe , ndipo zinthu zikuyendele bwino kuti umange nyumba ya Yehova Mulungu wako , monga mmene iye analankhulila za iwe . ” — 1 Mbiri 22 : 11 , 14 - 16 . Inde , mlongoyu anaika maganizo ake pa kucita cifunilo ca Yehova . 4 : 31 ) Makhalidwe amenewa amapangitsa munthu kukhala waciwawa . Tengelani Cilungamo ca Yehova na Cifundo Cake , Nov . Ngati mneneli wokhulupilika Mose anacenjenekewa mpaka kulakwila Mulungu , na ise zaconco zingaticitikile mosavuta . 34 : 18 , 19 . Komanso , ofalitsa ambili a kumeneko adzipeleka kukukila ku madela ena kuti akalalikile uthenga wa Ufumu m’gawo lonse la cisumbu cacikulu cimeneci . Kodi Munadyapo Mkate wa Moyo ? M’caka cotsatila , tinakhala na mwana wathu woyamba wamkazi , dzina lake Jane . Masako watumikila ku Russia kwa zaka zoposa 14 . Akaganizila zaka zimenezo , amanena kuti : “ Mavuto amene ndakumana nao sangapambane cimwemwe cimene ndapeza . 26 : 31 - 33 , 56 , 69 - 75 . ▪ Kodi Mumaona Dzanja la Mulungu pa Umoyo Wanu ? ( Mac . 18 : 4 , 5 , 26 ) Conco tiyenela kudzifunsa kuti , ‘ Kodi nimapewa kutamanda anthu ena mopambanitsa kapena kuseŵenzetsa nthawi yoculuka pa zinthu zosafunika kweni - kweni ? ’ — Ŵelengani Aefeso 5 : 15 , 16 . Tinali kukonda kulalikila m’madela osalalikidwa kaŵilikaŵili pamodzi monga banja Conco , muziphunzila Mau a Mulungu mwakhama ndi kusinkha - sinkha tanthauzo lake . Muziyesetsa kuonetsa cikhulupililo canu mwa kutengako mbali pa misonkhano ya mpingo . Mboni zimacita zimenezi cifukwa zimakhulupilila kuti zapeza coonadi . N’nali kukhala na amayi , na azikulu anga atatu . Mobweleza - bweleza , mneneli Yeremiya analangiza mfumu Zedekiya kuti aleke zoipa zimene anali kucita , koma sanamvele . Ndiyeno , zitseko za ndende zinatseguka . ( Salimo 90 : 10 ) Zimenezo n’zimene mtima wathu umalaka - laka . Mlongo wina dzina lake Lily anayesetsa kucita zimenezi . Mau a Mulungu amati : “ Uzilemekeza bambo ako ndi mai ako . ” ( Eks . Phunzilani ku Mbalame za M’mlenga - lenga 8 Koma pali maonekedwe ena ake amene amaonetsa kuti zipatso zonse ndi zakupsa . 15 : 3 ) Kodi zimenezi zitanthauza kuti iye amatiyang’ana kuti aziona ngati tiphwanya malamulo ake ? Koma anapeza cinthu camtengo wapatali comwe ndi ubwenzi wabwino ndi Yehova . Conco , nafenso tiyenela kuuzako ena kuti adziŵe ziphunzitso zofunika zimenezi . Satana ni mdani wathu . Anthu anga andiiŵala . ” — Yer . “ N’nali wokonzeka kugwila nchito iliyonse imene yapezeka , ndipo tinayamba kupewa kugula zinthu zosafunika kweni - kweni . ” — Jonathan Patapita zaka , n’namvela kuti atate asanamwalile , nawonso anali kuphunzila Baibo na Mboni za Yehova . Nkhaniyi ifotokoza cimene cinathandiza Yefita ndi mwana wake wamkazi kukhalabe okhulupilika ngakhale panthawi yovuta . Popeza kuti ma IUD okhala na mahomoni amapepukitsako cibalilo , nthawi zina madokotala amawaseŵenzetsa pothandiza akazi okwatiwa kapena osakwatiwa amene amataya magazi kwambili posamba . Nimakhala otopa , ndipo moyo wanga umadalila cabe mankhwala . Akakumana ndi mavuto amafufuza m’Mau a Mulungu kuti apeze njila yothetsela mavutowo . . . . Panthawi ya kampeni m’gawo losalalikidwa , tinakwela sitima kuyenda ku tauni ina m’mbali mwa mapili , ndipo tinacita lendi cipinda cina pa nyumba yogonamo alendo . Ena akaticitila zabwino , timaiŵala mwamsanga . N’nali kucitenga mopepuka . Coyamba , pamene anali na zaka pafupi - fupi 17 , abale ake anamugulitsa kuti akakhale kapolo . Mwina nthawi zina mumaganiza kuti Yehova anakusankhani kuti mudzapite kumwamba . Muzipatula nthawi yopumula tsiku lililonse . Iye anakamba kuti : “ Zinthu zina zimanivuta kujaila , koma ngakhale kuti sinikwanitsa kucita zambili , nimaona kuti ndine wofunika mu mpingo . 2 : 20 ) Paulo anakhulupililadi dipo , ndipo anazindikila kuti limagwilanso nchito kwa iye . Ciphunzitso cimeneci cimakambanso kuti zimene apapa amaphunzitsa n’zodalilika . Kodi mukumva bwanji kudziŵa kuti mapeto ali pafupi ? Pamene Yesu anakamba kuti : “ Ngati Mwana wakumasulani , mudzakhaladi omasuka , ” anali kukamba za kumasuka ku ‘ ukapolo wa ucimo , ’ umene wasautsa anthu kwambili kuposa ukapolo wina uliwonse . Pambuyo pakuti Mfumu Asa wagonjetsa gulu la nkhondo la Aitiyopiya , mneneli wa Mulungu , Azariya anapatsa Asa ndi anthu ake uphungu wothandiza . Pa nthawiyo , Haykanush ndi mwamuna wake analibiletu ndalama ndiponso anali ndi nkhongole . Kweni - kweni , amenewo ni anthu otsatila zokhumba ndi zilakolako zawo , kaya ni zaciwelewele kapena zina . Cionjezeko cimeneci n’cogwilizana ndi ulosi wakuti : “ Wamng’ono adzasanduka anthu 1,000 , ndipo wocepa adzasanduka mtundu wamphamvu . Iye ananenanso kuti : “ Koma tinali ndi mantha . Mu mzinda wonse , anthu anacita cikondwelelo cacikulu cacipambano cimene cinali cikalibe kucitikapo mu mzinda waukulu umenewo . ( Ŵelengani Mateyu 4 : 4 - 10 . ) ( 1 Akorinto 13 : 8 ) Conco , masiku ano sitiyenela kuyembekezela kuti Mulungu adzaticilitsa kapena kucilitsa okondedwa athu mozizwitsa . Ambili a ife tinakambapo mau oipa kapena kucita zinthu zosayenela cifukwa copupuluma , ndipo pambuyo pake tinadziimba mlandu . — Miy . Pa nthawi yocepa cabe , nyumba zoposa 40,000 zinadzala madzi , kuphatikizapo nyumba zambili za abale athu . Pali zinthu zina zimene Akhristu ena amacita , zoonetsa kuti sanasiiletu khalidwe la kudziko . Tikatelo , tidzatsimikiza mtima kupewa magazi . Nyimboyi ndi yokhudza cikondi ca pakati pa mtsikana wa ku mudzi wina wochedwa Sunemu , kapena kuti Sulemu , ndi m’busa wacinyamata . 12 : 40 - 42 ; Agal . Komabe , pamene anthu aŵili agwilizana ndi kumanga banja , aliyense afunikila kusintha . 22 : 15 ) Conco , popeza kuti munthu wanzelu sacita zinthu mwaucitsilu , ndiye kuti nzelu n’cizindikilo cakuti munthu ni wacikulile kuuzimu . Lamulo lamphamvu lolola Mboni za Yehova kuti zidzilambila mwaufulu linakhazikitsidwa . ( Afil . Iwo anali kupita kulikonse kumene kunali kupezeka anthu . Koma coyambilila tiyenela kupita kukalalikila kwa anthuwo . Conco , kulekanitsa nkhosa ndi mbuzi kuyenela kucitika Ulamulilo wa Zaka 1000 usanayambe . 6 : 15 - 17 ) Komabe , anthu a Mulungu adzathaŵila ku malo acitetezo ophiphilitsa amene Yehova adzapeleka . Mlongoyu anati : “ Makolo anga sanandilangepo ali okwiya kapena popanda kundiuza cifukwa cake akundilanga . ” Komabe , zimene akanasankha zikanawacititsa kukhala ndi moyo kapena kufa . Yehova anadalitsa Yakobo kwambili . Nafenso tifuna kuti Mulungu atidalitse . 15 : 5 - 7 ) Mwa cikhulupililo , anthu oopa Mulungu amenewo ‘ anaona ’ mbadwa zao zikukhala m’dzikolo . Alambili onse a Yehova ayenela kumvela malangizo opezeka m’Mau a Mulungu . Akatelo adzapewa ‘ kumvetsa cisoni mzimu woyela . ’ ( Aef . 31 Kuonetsa Kukoma Mtima Kamodzi Cabe Yehova adziŵa zimene tifunikila , ndipo watipatsa cakudya cokwanila kuti tikhale olimba kuuzimu . — Mat . 3 , 4 . ( a ) Ndi liti pamene Ophunzila Baibulo anayamba kudziŵika ndi dzina latsopano ? Kodi Cidzacokapo N’ciani Ufumu wa Mulungu Ukadzabwela ? Nanga tingaonetse bwanji cikondi kwa mnzathu ? Pakapita mphindi 30 , nesi wamwamuna anali kundipima kuti aone mmene magazi anga anali kuyendela . Baibo imakamba kuti : “ Mtembowo utangokhudza mafupa a Elisa , munthuyo anakhalanso wamoyo ndipo anaimilila . ” ( 2 Maf . Cifukwa “ sanatsimikize kufunafuna Yehova ndi mtima wake wonse . ” — 2 Mbiri 12 : 14 . Rabeka anaona mmene mwamuna wacikulile anali kumuyang’anila . Kodi Nyimbo ya Solomo imatiphunzitsa ciani pankhani ya cisumbali ? N’cifukwa ciani kucotsa munthu wosalapa mumpingo ndi makonzedwe acikondi ? Mulungu anafotokoza cimene cinapangitsa . Yesu anatsimikizila ophunzila ake kuti ngati adzaika Ufumu patsogolo , Mulungu adzawathandiza . Kodi nafenso tingathe kukhala pa ubwenzi wolimba ndi Yehova ? Kodi mumacita mantha kucita ulaliki wa poyela ? “ Anthu anu amene anafa adzakhalanso ndi moyo . Kale , kuti Yehova atsogolele ndi kulinganiza anthu ake , anali kuseŵenzetsa anthu omuimila . Tonse timafuna kucita zimene Baibulo limakamba . ( Mateyu 5 : 43 - 45 ) Popeza ndife atumiki a Mulungu , tiyenela kukonda adani athu mosasamala kanthu za zimene amaticitila . ( Aroma 15 : 4 ) Conco , ni cinthu canzelu kuŵelenga nkhanizi , kuziphunzila , na kuzisinkha - sinkha . ( Danieli 2 : 44 ) Baibulo limati : “ Koma anthu ofatsa adzalandila dziko lapansi , Ndipo adzasangalala ndi mtendele woculuka . ” — Salimo 37 : 11 , 29 . Kulinso mipingo 11 komanso magulu atatu amene amagwilitsila nchito cinenelo camanja ca ku Honduras Kumeneko anakapatsidwa nchito yowonjezeleka . “ Anamuika pamwambamwamba kuposa boma lililonse , ulamulilo uliwonse , amphamvu onse , ambuye onse . ” ( Aef . 11 ) Ndithudi , cimeneci n’cifukwa comveka copitilizila kucita zabwino . N’ciani cionetsa kuti zolengedwa zauzimu nthawi zonse zimagwila nchito yokondweletsa ndi yokhutilitsa ? Koma mwacionekele zimene anauza Timoteyo zinam’thandiza kudalila Yehova kwambili . Abale ndi alongo athu mumpingo naonso ndi anzathu . Akhristu ena oyambilila anakhudzidwa ndi mzimu wokonda zinthu za m’dziko . Mphatso zina ni za mtengo wapatali cifukwa ca zimene wopelekayo watailapo . Ku Sierra Leone , mu 1982 Timapindula bwanji ngati tili na “ mtendele wa Mulungu ” ? Koma analimbikitsidwa kwambili na mau a Yesu apa Mateyu 19 : 26 , pamene pamati : “ Zinthu zonse n’zotheka kwa Mulungu . ” Ndiyeno , ndinasankha kusangalatsa mtima wa Yehova . Koma malinga ndi zimene takamba kuciyambi kwa nkhani ino , sitidziŵa bwinobwino mmene Satana anaonetsela Yesu kacisi . ndi kulimbikitsakonso ena kucita zimenezi ? Mosakayikila , pamene abale a ku Filipi anaŵelenga kalata imene Paulo anawalembela , anakumbukila mavuto amene iye anakumana nawo , ndiponso zinthu zosayembekezeleka zimene Yehova anamucitila . Tonse tifunika kutsatila mfundozi mosasamala kanthu za nyengo , cikhalidwe , kapena dela limene tikhalako . Mwacitsanzo , Paulo anacha Timoteyo kuti “ mwana wanga wokondedwa ndi wokhulupilika mwa Ambuye , ” amene anali kudzasamalila zosoŵa za Akhiristu na mtima wonse . ( 1 Akor . 4 : 17 ; Afil . Mulungu anapatsanso Adamu udindo wopatsa maina nyama zonse m’munda wa Edeni . Ndiponso , kapolo wokhulupilika amaika oyang’anila dela ndi abale a m’Komiti ya Nthambi . 22 : 22 . ( Salimo 104 : 24 ; Machitidwe 14 : 17 ) Yehova amachela khutu , ndipo amasangalala akationa kuti tikusinkhasinkha , kupemphela , ndi kuuzako ena za iye . Pofotokoza nkhondo yoyamba ya pa dziko lonse imene inali kucitika ku Ulaya , Nsanja ya Mlonda yacingelezi ya September 1 , 1915 inati : “ Nkhondo zonse zimene zinacitika m’mbuyomu , zinali zazing’ono kuyelekezela ndi nkhondo imeneyi . ” Baibo imatiuza kuti : “ Yehova Mulungu anameletsa m’nthaka mtengo wamtundu uliwonse wooneka bwino ndi wa zipatso zabwino kudya . ” Pa ulendo wawo wolalikila m’madela akutali m’dziko la Australia , Arthur Willis ndi Bill Newlands , amene tachula kuciyambi kwa nkhani ino , anavutika kwambili kwa mawiki aŵili pa ulendo wawo wa makilomita 32 , cifukwa mvula yamphamvu inacititsa kuti m’cipululu mukhale matope okha - okha . BAIBO SI BUKU LOPHUNZITSA ZA MATENDA , KOMA ILI NA MALANGIZO OTSOGOLA PA ZA UMOYO . Pemphelo ndi mwai wapadela kwambili ! Ndipo Malemba Aciheberi anali ndi maulosi ambili onena za Mesiya . N’cifukwa ciani tiyenela kuyesetsa kukhala na “ maganizo a Khristu ” ? Ndinasoŵa cokamba moti ndinangoti , Mhhu ‘ Akristu aŵa ndi a mtundu wina ! ’ N’ciani cimene tingacite kuti tipeze cimwemwe ceni - ceni ? Hans anafotokoza kuti : “ Popeza tinali kufuna kuyenda kumene Yehova afuna , tinamupempha kuti atitsogolele . Pamene Mose anali kutonzedwa , kodi cikhulupililo cinam’thandiza bwanji kuona utumiki wake kukhala wofunika ? Atumiki anga adzafuula mokondwa cifukwa cokhala ndi cimwemwe mumtima . ” ( Yes . Bungwe la akulu lililonse lili ndi udindo wopenda mosamalitsa ziyeneletso za m’Malemba za abale amene asankhidwa kuti aikidwe pa udindo mumpingo . M’zaka 100 zoyambilila , atsogoleli azipembedzo anali kutsutsana pa nkhani yothetsa cikwati . Cinanso n’cakuti anthufe tinalengedwa na cikumbumtima . Cikumbumtima cimeneci , ngakhale kuti nthawi zina cimakhala copotoka , cimatithandiza kudziŵa cabwino ndi coipa , kapena colungama ndi cosalungama . Panthawi inayake , kumwamba kunalibe mtendele . Kumeneko n’nakumana na mayi wina amene ananipempha kuti niziphunzila Baibo ndi ana ake aakazi ogontha , Jean na Joan Rothenberger , amene anali amphundu . Ndikali wamng’ono , atate anga anazindikila kuti ndikangomva nyimbo ikulila ndinali kuvina . M’zaka za posacedwapa , gulu la Yehova lakhala likupeleka malangizo akuuzimu osavuta ndi omveka bwino . Anthu ambili amamvela monga mmene Doreen anamvelela . Ŵelengani kuti mudziŵe zimene zinawacitikila pambuyo pakuti ndalama zao zatha , pamene anali kutumikila monga amishonale ku India . Ciyembekezo canga cili mwa inu tsiku lonse . ” ( Yoswa 10 : 13 ) Koma Yehova analola adani a Isiraeli “ kuumitsa mitima ” yao kuti acite nkhondo ndi Isiraeli . Eric na Amy 12 : 23 , 24 ) Mofananamo , Yehova amasamalila aliyense wa ife , mosayang’ana zofooka . N’zoona kuti tonsefe timafuna kulimbikitsidwa . Lomba , akusamalila amayi ake ku Canada , ndipo akutumikila monga mpainiya wapadela . Phunzilo la Baibulo linakhazikitsidwa , ndipo pano tikamba mnyamatayo ni m’bale . ‘ Kodi pali zinthu zina zimene ndingasinthe kuti nditsatile Yesu mosamala kwambili ? ’ Ndipo mwina makolowo angafunikile cisamalilo kwa kanthawi kapena kwa nthawi yaitali . Nayenso Fern wa zaka 91 , wa ku Brazil anati : “ Pakapita nthawi ndimagula zovala zatsopano n’colinga cakuti ndizioneka bwino . ” Amatsimikiza kuti olambila oona akukhala na cakudya cauzimu ca mwana alilenji m’paradaiso wauzimu . ( Yes . Usagwilizane ndi munthu woipa mwa kukhala mboni yokonzela wina zoipa . ” — Ekisodo 23 : 1 . * Kodi nanunso mumamva conco ? Ndani ayenela kudya zizindikilo ? ( Chiv . 19 : 20 , 21 ; 20 : 9 ) Conco , n’zosadabwitsa kuti anthu onse amene adzapandukila Mulungu pambuyo pa Ulamulilo wa Zaka 1,000 amachedwa “ Gogi ndi Magogi . ” ( Gen . 22 : 15 - 18 ) Ndiponso , nthawi zonse Yehova amaseŵenzetsa ufulu wake mogwilizana ndi makhalidwe ake a cikondi na cilungamo . 4 : 13 ; Mat . 4 : 1 - 3 ) Mtendele umene uli “ monga comangila cotigwilizanitsa , ” ndi wamtengo wapatali . Kodi Tingapeze Kuti Citonthozo ? Nowa ayenela kuti anaphunzila za cikhulupililo ca Inoki , kucokela kwa Lameki , atate ŵake , kapena kucokela kwa Metusela , ambuye ake . N’kuthekanso kuti anaphunzila zimenezi kwa Yaredi , atate a Inoki , amene anamwalila pamene Nowa anali na zaka 366 . — Genesis 5 : 25 - 29 ; 6 : 9 ; 9 : 1 . Iye anakamba kuti : “ Ciyembekezo ca Paladaiso cimanithandiza kuika zolinga zakuthupi pa malo oyenelela . Poyamba sin’nali kudziŵa kuti ningakhale na umoyo monga umene nili nawo kuno . Iye anali kudziŵa kuti mtengo ukadulidwa , umaphukanso n’kukhala ngati watsopano . 21 : 3 , 4 ) Sitikukaikila kuti kudzela mwa Kristu , Yehova adzalamulila mphamvu zacilengedwe m’zaka 1,000 za ulamulilo wa Yesu . N’zoonekelatu kuti kuganizila malonjezo a Mulungu n’kumene kunathandiza Abulahamu kukhala ndi cikhulupililo camphamvu . Ndiyeno , citani zinthu ‘ mwanzelu . ’ Mwa kuthandiza Mose ndi mzimu woyela , Yehova anapitiliza kutsogolela anthu Ake . Ngakhale n’conco , anali kutopa ndipo anafunikila kupumula cifukwa cogwila nchito mwakhama . — Luka 8 : 23 ; Yohane 4 : 6 . Banja lathu linali la Katolika ndipo tinali kukonda kwambili kupemphela . Iye anati : “ Koposa zonse , naona kuti ubale wanga ndi Yehova umanipatsa mphamvu zolimbana na nkhawa zanga . Komabe , zimene Paulo analemba m’caputa 7 zimatithandiza kumvetsa zimene “ thupi ” lochulidwa pa Aroma 8 : 4 - 13 limatanthauza . Iye adzakhala ciliconse cimene angafune kuti akwanilitse cifunilo cake Ambili mwa io ndi akazi ndi ana . Bungwe Loona za Umoyo pa Dziko Lonse linacenjeza kuti : “ Ngakhale anthu amene amapumako cabe utsi umene umatuluka wina akamakoka amakhala pangozi . ” Pali Mboni za Yehova zoposa 8,000,000 m’mipingo yoposa 115,400 padziko lonse , ndipo ciŵelengelo cikuonjezeka . Pamene anali padziko lapansi , Yesu analalikila m’madela ocepa kwa zaka zitatu ndi hafu . ( Mat . ( Miy . 18 : 11 ) Koma kukhala na cidalilo conse cakuti Yehova adzakusamalilani , kungakuthandizeni kupilila nkhawa , kapena kuzipewa . Koma iye sanadzionetsele . 10 , 11 . ( a ) N’ciani cidzacitikila anthu oipa ? Amai anga enieni sindinali kuwadziŵa ndiponso sindinali pa ubwenzi wabwino ndi atate anga . Nkhani ino yakulimbikitsani kuika mtima wanu wonse pa kutumikila Yehova . Nanga kudziŵa zimenezi kumakhudza bwanji ubwenzi wathu ndi Iye ndiponso ubwenzi wathu ndi abale ndi alongo athu ? Mmene Mkristu amagwilitsila nchito cikumbumtima cake , zimaonetsa kuti ndi wofikapo kuuzimu kapena ai . Mwacitsanzo , mkulu wina wacicepele dzina lake Jason , anati : “ N’tangoikidwa kukhala mkulu , n’nali kuona kuti siningakwanitse kusamalila udindowu . ” Pamene anali na zaka 12 , aphunzitsi pa kacisi anadabwa kwambili na ‘ mayankho ake komanso poona kuti anali womvetsa kwambili ’ zinthu zauzimu . — Luka 2 : 42 , 46 , 47 . Iwo anagwidwa ukapolo m’caka ca 740 B.C.E . , pamene mafuko 10 a Aisiraeli amene anali kupanga ufumu wa kumpoto , anagwidwa ukapolo ndi kucoka m’dziko lao . Iwo sanali kulambila mulungu wa mwezi wochedwa Sini . Yehova , Atate wathu wakumwamba , ndiye anatipatsa moyo . Tinasangalala titaona kuti akukalamila maudindo mumpingo . Koma Yesu anasumika maganizo ake pa zimene mtumikiyu anacita , osati pa mlandu umene anafuna kum’cotsela nchito . Mfumu Davide inalemba kuti : “ Zakumwamba zikulengeza ulemelelo wa Mulungu . Maso a Jairo nthawi zonse amayang’ana mwacidwi ndikamamuŵelengela lonjezo la m’Baibulo lakuti : “ Munthu wolumala adzakwela phili ngati mmene imacitila mbawala yamphongo . Mwacitsanzo , M’bale Gardner atangodziŵa kuti ndinali kugona m’galimoto , anapita nane kwa mlongo wina amene anali ndi nyumba yogona alendo . Pamene n’nali wacicepele , makolo anga nthawi zambili anali kuitana oyang’anila dela ndi akazi awo kuti tikakhale nawo kunyumba kwathu kwakanthawi . Coyamba , Yehova anatsimikizila Mose kuti : “ Ndidzakhala nawe . ” Baibo imaonetsa kuti pambuyo pa Ulamulilo wa Khristu wa Zaka 1,000 , anthu ena adzapandukila ulamulilo wa Yehova . ( Chiv . Cifukwa cokonda okalamba amenewa , Akristu ena amadzipeleka kuti awathandize mmene angathele . Kodi mwalimbikitsidwa bwanji ndi zimene Mfumu Mesiya wakwanitsa kucita mkati mwa ulamulilo wake wa zaka 100 ? Ndithudi , Yehova wanithandiza m’njila zambili . Sananigwilitsepo mwala . Pamene tinamaliza kuyendela mipingo yonse m’dela limene tinapatsidwa , ofesi ya nthambi inatitumila foni . ( Machitidwe 11 : 26 ) Iwo sanali kufunikila dzina lina lapadela cifukwa Akhiristu onse anali ndi cikhulupililo cimodzi . Mwakucita zimenezi , Gidiyoni anaonetsa kuti anali wocenjela kwambili . M’malomwake , anali kukamba za kukola nsomba pogwilitsila nchito maneti . Nkhani ziŵilizi zifotokoza mmene timapindulila ndi kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova . Mtumwi Paulo anafotokoza kuti : “ Wobyala mooloŵa manja adzakololanso zoculuka . ” 4 : 10 . Zimenezi zimalimbikitsa a nkhosa zina kupitilizabe kugonjela Mfumu yao yaulemelelo ndipo io amayamikila mwai umene ali nao wogwilizana ndi otsalila a odzozedwa padziko lapansi . “ Munavomeleza Kuti Zimenezi Zicitike ” Amuna ena amaletsa akazi awo acikhristu kuphunzitsa ana Baibo . 45 : 5 - 8 ) Iye sanaimbe mlandu Yehova pa zimene zinamucitikila . Ici n’cizindikilo coyenelela kwambili coonetsa mmene miyezo yolungama ya Yehova imatetezela mtima wathu wophiphilitsa . Anita Kodi lemba la Salimo 41 : 3 lingatilimbikitse bwanji ? Nawonso anthu apabanja , amene amakonda ulamulilo wa Yehova angatengele citsanzo cake . Pambuyo pake , msilikaliyo anakhulupilila , koma anamuuza kuti alipile ndalama yandapusa cifukwa cosakhala na ziphaso zoyenelela . Tiyenela kupemphela kuti iye atipatse mzimu woyela , umene ungatithandize kukhala oleza mtima ndi odziletsa . Sititengamo mbali m’ndale za dziko ndipo sitinyamula malupanga . ( Mat . Iye analinso membala wa Khoti Lalikulu la Ayuda . — Yoh . 3 : 1 - 10 ; 7 : 50 - 52 . Ndipo nthawi ndi nthawi amayesetsa kuwacezela . Koma ao amene amakhala pafupi ndi makolo angathandize amene ali mu utumiki wanthawi zonse . Zimene Yesu ndi atumwi ake anali kuphunzitsa , n’zothandiza kwambili masiku ano monga mmene zinalili m’nthawi ya atumwi . 13 Mbili Yanga ​ — Tinaona Cisomo ca Mulungu m’Njila Zambili Pambuyo pakuti Petulo wacilitsa munthu amene anabadwa wolemala , amunawo anafuna kuti Petulo afotokoze kuti anacita zimenezo ndi ulamulilo uti kapena m’dzina la ndani . Modzicepetsa , iye anati : “ Ndinamva zimene ananenazo , koma sindinadziŵe tanthauzo lake . ” Zimenezi zingakhalenso zoona ndi inu . Koposa kale lonse , “ mapeto a zinthu zonse ayandikila ” kwambili . ( 1 Pet . Popeza ndiwe fumbi , kufumbiko udzabwelela ’ ” — Genesis 3 : 17 , 19 . Nanga n’cifukwa ciani Yesu anapita kumeneko popeza anali wangwilo ndiponso sanali kudwala ? Dziko lonse linafunikila kudziŵa za cigololo ca Babulo Wamkulu . Masiku ano , atumiki a Mulungu samenya nkhondo yeni - yeni . Nafenso Yehova adzayankha mapemphelo athu ocokela pansi pamtima , malinga ngati ‘ tilimbikila kupemphela . ’ — Aroma 12 : 12 . 18 : 1 - 8 ; 1 Tim . Mmene Timavalila Umunthu Watsopano ndi Kusauvulanso , Aug . 18 : 1 ) Tiyenela kukonda Mulungu cifukwa cakuti nayenso amatikonda . Kodi Aisiraeli anadziŵa bwanji kuti Mose anali na mzimu wa Mulungu ? Satana akadzacotsedwa , mavuto amene anayambila pa Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse adzatha . N’CIFUKWA ciani ndinu wotsimikiza mtima kuti Yehova amakonda anthu ake ? ( Zefaniya 2 : 13 - 15 ) Kodi akatswili a mbili yakale atulukila ciani ? ( 2 Tim . 3 : 1 ) Kupanda cilungamo , matenda , ulova , imfa , ndi mavuto ena , pang’ono m’pang’ono zingacititse ena kukhala opanda cimwemwe . Ena anawaganizila kuti acita misala . Mmodzi wa iwo anali Gustav Kujath , amene anapelekedwa ku cipatala ca amisala . Anasonkhanitsa amuna olimba mtima okwanila 10,000 kuti akamenyane ndi gulu lankhondo loopsa la Sisera . Cigumula citayamba mu 2370 B.C.E . , Yehova “ anaseselatu camoyo ciliconse cimene cinali padziko lapansi , ” koma anasunga Nowa ndi banja lake . ( Gen . Anthu amene amatsatila mfundo za m’Baibulo agonjetsa kusankhana mitundu ndipo amalambilila capamodzi . Conco , tikulimbikitsani kumapatula nthawi yophunzila za Yehova Mulungu amene anapeleka “ mphatso yangwilo , ” ndi zimene mufunika kucita kuti mukasangalale na moyo wosatha , umene udzatheka cifukwa ca dipo la Yesu . ( Sal . 68 : 11 ) Kodi mungasinthe zinthu zina kuti mutsatile mapazi a alongo acangu amene anafunsidwa mafunso m’nkhani ino ? Mwacitsanzo , mpukutu wa Yesaya umene unapezeka pa Mipukutu ya m’Nyanja Yakufa , ni wakale kwambili na zaka 1000 kuyelekezela na mau a m’mipukutu ina imene ilipo kale . Pambuyo pa masiku 40 Yesu atabadwa , Mariya anapita ku kacisi ku Yerusalemu kukapeleka nsembe kwa Yehova . Uwu unali ulendo wa makilomita 9 kucokela ku Betelehemu . VUTO LIMENE LINALIPO : Olemba Baibulo ndi okopela malemba , nthawi zambili anali kuseŵenzetsa gumbwa ndi zikopa ( zikumba ) za nyama . Tikhoza kuona mmene tingazigwilitsile nchito m’banja , ku nchito , ku sukulu , kapena mu ulaliki . Nanga n’ciani cimene ife tiyenela kucita kuti tisaumitse mitima yathu n’colinga cakuti tipindule ndi zimene Yesu anali kuphunzitsa ? Kodi makolo ayenela kuonetsetsa ciani ? Tinenenso kuti mnzanu wa muukwati wakufunsani kuti , “ N’cifukwa ciani simunandiuze zimene munakonza kudzacita pa Ciŵelu ? ” ( b ) Yehova amamva bwanji tikamauzako ena za iye ? Sitingakwanitse kuchula zinthu zonse zimene Yehova amaticitila cifukwa ca cikondi cake cosatha . Ngati Bungwe Lolamulila limalola Mau a Mulungu kutsogolela zosankha zawo osati maganizo ofala a anthu , n’ndani kweni - kweni amene atsogolela anthu a Mulungu masiku ano ? ( Onani pikica kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Kodi angelo anathandiza bwanji bungwe lolamulila ? Ndipo cimodzi mwa zinthu zimene zinanithandiza kuti niyamba upainiya ndi cilimbikitso cawo . Yesu anauza Mulungu m’pemphelo kuti : “ Moyo wosatha adzaupeza akamaphunzila ndi kudziŵa za inu , Mulungu yekhayo amene ali woona , ndi za Yesu Khristu , amene inu munamutuma . ” ( a ) N’ciani cidzacitikila dongosolo la zamalonda la m’dzikoli ? Lomba nikuphunzila na atsikana 5 mwa atsikana amenewo . ” Vesili ndi lofunika kwambili cakuti ena amanena kuti uthenga wonse wabwino upezeka m’vesi limeneli . Koma pa Sondo , pa December 18 , 2011 , zinali zokondweletsa kwambili kuona abale athu oposa 78,000 a mitundu yosiyana - siyana ocokela ku South Africa ndi maiko ena apafupi , atasonkhana pamodzi . Iwo anasonkhana m’sitediyamu yaikulu mumzinda wa Johannesburg , kuti asangalale ndi pulogilamu yauzimu . Pamenepo adzaweluzidwa “ mogwilizana ndi nchito zao , ” kuona ngati anali kumvela malamulo a Mulungu kapena ai . Mwacitsanzo , tiyeni tiganizile kumene tikhala . Njila imodzi imene iye amacitila zimenezi ndi kuyang’ana kacizindikilo pa kompyuta yake kamene kamaonetsa munda umene nyama ndi anthu a mitundu yonse adzakhala mwamtendele . Nkhani ya mkazi wamasiye wosauka itiphunzitsa kuti Yehova amaona ndipo amayamikila zilizonse zimene timam’citila , maka - maka ngati tizicita panthawi zovuta . Yesu anafotokoza mwafanizo mmene Mulungu amatisamalila . 2 : 44 ) Kwa zaka zambili ophunzila Baibo anali kunena kuti caka ca 1914 cidzakhala capadela . Lomba sinivutikanso maganizo komanso sinivutitsanso ŵena . Nchito yapadela imene inacitika ku Turkey , inathandiza kuti anthu ambili amvele uthenga wabwino . Mpaka pano , Paula akutumikilabe Mulungu mokhulupilika . ( Yobu 39 : 27 - 29 ) Maso a ciwombankhanga ndi amphamvu kwambili cakuti cingathe kuona kalulu ali pa mtunda wokwana kilomita imodzi . Limatitonthoza ndiponso kutipatsa ciyembekezo ndi malangizo othandiza . Mau amenewa sanathetseletu cisoni ca Marita . Koma iye anakhulupilila zimene Yesu anakamba . Mogwilizana ndi tanthauzo la dzina lake , Yesu anathandiza “ nkhosa zosocela za nyumba ya Isiraeli ” kulapa macimo ao kuti Yehova awalandilenso . ( Mat . Tilinso na cifukwa cina copitilizila kugwila nchito yolalikila . Inde , umunthu wanu umaphatikizapo zonse zokhudza imwe . Solomo anagwilitsila nchito mau a ndakatulo ocititsa cidwi pofotokoza mavuto amene okalamba amakumana nao monga kunjenjemela manja , kuyenda mwapenda - penda , kuguluka manu , kusaona bwino , kuvutika kumva , imvi , ndi kuyenda moŵelama . Iye amati : “ Mudzaitanila pa ine komanso mudzabwela ndi kupemphela kwa ine ndipo ine ndidzakumvetselani . ” Tanthauzo limeneli limuyenelela Yehova popeza ndi Mlengi wacilengedwe conse ndi wokwanilitsa malonjezo . Mosakaikila , citsanzo cabwino ca Yakobo ndi Rakele cinathandiza mwana wawo Yosefe . Anaphunzila zimene angacite pokumana ndi mavuto oyesa cikhulupililo cake . Pa cifukwa cimeneci , panafunika kukulitsa ofesi ya nthambi , ndipo n’zimene zinacitika mu 1988 . Mungayambe kukamba naye mwa kunena kuti : “ Mwina ine n’nangofulumila kukwiya , koma pamene munakamba na ine dzulo , n’namva monga . . . N’nayamba kudziona kuti ndine wacabecabe ndiponso wonyansa . Ndimakonda kwambili banja langa ndipo ndimacita zinthu zimene zimalisangalatsa . Zioneka kuti panthawi yovutayi ndi pamene Paulo anaikidwa m’ndende kaciŵili ku Roma . Imfa Si Mapeto a Zonse Ni khalidwe loipa cifukwa nkhawa imawonjezeka , ndipo zimacititsa munthu kusacita bwino nchito . ” “ Akazi amene akulengeza uthenga wabwino ndi khamu lalikulu . ” — SAL . Mmodzi wa iwo ndi mzimayi wa zaka 67 . 22 : 2 ) Lamulo limeneli liyenela kuti linamukhudza ngako Abulahamu . Kodi mitunduyo idzatsogoleledwa ndi “ mfumu ya kumpoto ” yophiphilitsa ? Ndani anafunika kuona nchito yao ? Iwo amavala zovala zothina ndi zoonetsa thupi , ngakhale popita ku misonkhano . Cinali kumveka monga “ makeke opyapyala othila uci , ” ndipo cinali cokwanila kwa onse . Ngati mufuna kupanga cosankha cofunika , nthawi zonse muzidzifunsa kuti : ‘ Kodi cosankha canga cidzaonetsa kuti nimakonda Yehova ? 20 : 24 ) N’zoonekelatu kuti Paulo sanacite mantha cifukwa cakuti adzakumana ndi mazunzo . Ŵelengani Yohane 3 : 16 . 14 : 4 ) Motelo , tikamatsatila malangizo awo , ndiye kuti tikutsatila Mtsogoleli wathu , Yesu . ( Mat . 26 : 52 , 53 ) Mfundo yamphamvu imeneyi ni yogwilizana ndi pemphelo limene iye anapeleka madzulo a tsikulo , lakuti ophunzila ake sayenela kukhala mbali ya dziko . Yehova amayembekezela kuti munthuyo adzakwanilitsa lonjezo lake . Nafenso ndife opanda ungwilo . 11 : 7 ) Abulahamu na Sara nawonso anatsatila citsogozo ca Mulungu kupita ku dziko lolonjezedwa . Ndipo kumwamba kunamveka mawu osiyanasiyana , akunena mokweza kuti : ‘ Ufumu wa dziko wakhala ufumu wa Ambuye wathu ndi wa Khiristu wake . Iye adzalamulila monga mfumu kwamuyaya . ’ ” — Chivumbulutso 11 : 15 . Kodi cisautso cacikulu cidzayamba bwanji ? Nanga zimenezi zidzacitika bwanji ? Conco , kodi mtumwi Paulo anali kukamba ciani pamene anati : “ Aliyense wochula dzina la Yehova aleke kucita zosalungama ” ? Katswili wina wa Baibulo anacha ulalikiwu kuti “ nkhani yothandiza , ” ndipo anakamba kuti colinga ca ulalikiwo ndi “ kutitsogolela paumoyo wathu , osati kutidziŵitsa zinthu zosiyanasiyana . N’nadzimva kukhala wacabe - cabe , n’nalibe mphamvu , n’nalibenso tsogolo . ” Pamenepo ophunzilawo anati : ‘ Ambuye , ngati iye akupumula , apeza bwino . ’ Iye anapitiliza kuti : “ Ndinali kukhalila kusamukasamuka cakuti sindingakumbukile nthawi zimene ndinauzidwa mwadzidzidzi kuti ndicoke m’nyumba . ” Yesu anayamba kufunsa mafunso ofunika akali ndi zaka 12 cabe . Cimakamba za zolengedwa zauzimu za kumwamba zimene zimafuula potamanda Yehova , “ amene adzakhalabe ndi moyo kwamuyaya . ” Anadziŵa kuti kulambila konama , kuphatikizapo kukonda cuma , ‘ n’kukana Mulungu woona wakumwamba . ’ Komabe , tiyenela kupewa maganizo akuti , “ Zinthu zanga ndi za m’dziko langa ndiye zabwino kuposa zonse . ” Pamene tiphunzila nkhani ino monga mpingo , tili mkati moitanila anthu ambili ku Cikumbutso ca imfa ya Khiristu . Ponena za cisautso cacikulu , cimene tsopano cayandikila , Yesu anati : “ Cizindikilo ca Mwana wa munthu cidzaonekela kumwamba . Ndiyeno mafuko onse a padziko lapansi adzadziguguda pa cifuwa cifukwa ca cisoni , ndipo adzaona Mwana wa munthu akubwela pa mitambo ya kumwamba ndi mphamvu ndi ulemelelo waukulu . Olo kuti cikhulupililo n’cofunika , cidzatha panthawi imene tidzaona kukwanilitsika kwa malonjezo a Mulungu ndi kuona kuti zimene tinali kuyembekezela zacitika . Koma kukulitsa cikondi kwa Mulungu ndi kwa anzathu sikudzatha . Kodi n’zotheka kuti Mkristu wodzozedwa alephele kukhala maso panthawi imene akuyembekeza kubwela kwa Kristu ? Inde , cifukwa timacitila umboni za Ufumu wa Yesu . Mlongo Cathy avomeleza kuti cikwati cimafuna munthu kusintha . Iye anati : “ Pamene n’nali mbeta , n’nali kungocita zimene nikufuna . Pamene cigaŵenga catsala pang’ono kunyongedwa , anthu ena angacite zionetselo za kusakondwa ndi ciweluzoco . 9,040 Mu December 2011 , mvula yamkuntho inapangitsa kuti madzi asefukile pa cilumba ca Mindanao ku Philippines . Koma ndife otsimikiza kuti : Anthu omvela adzakhala ndi cimwemwe , cifukwa Yehova adzakhutilitsa zosoŵa ndi zokhumba zao zonse m’njila yabwino koposa . — Sal . Ndipo Adamu anaonetsa mtima wodzikonda pofuna kukondweletsa Hava . Pambuyo polinganiza bwino zinthu komanso cifukwa cothandizidwa ndi ana athu asanu , Lidasi naye anayamba utumiki wa nthawi zonse mu 1960 . Maumboni onse akuonetsa kuti mu 1919 , Akristu odzozedwa anamasulidwa ku ukapolo wa Babulo Wamkulu , ndipo anasonkhanitsidwa mumpingo woyeletsedwa . Kodi cikumbumtima cathu tingaciphunzitse bwanji ? Atsogoleli a maiko analonjeza kuti nkhondo idzathandiza kuti zinthu zikhale bwino padziko . Ali koceza , anacita ngozi yoopsa kwambili pagalimoto , ndipo zimenezi zinacititsa okondedwa ao ndi anzao akunchito kumva kuti cinacake cinali kusoŵeka pamoyo wao . Dzina la Mulungu lakuti Yehova , Malinga ndi kafuku - fuku wina , “ munthu mmodzi angasonkhezele anthu ambili - ambili kukhala opatsa , ngakhale anthu amene sawadziŵa kapena amene sanawaonepo . ” Zimenezi zitikumbutsa zimene Yakobo analemba . Iye anati : “ Ngati m’bale kapena mlongo ali waumphawi ndipo alibe cakudya cokwanila pa tsikulo , koma wina mwa inu n’kunena kuti : “ ‘ Yendani bwino , mupeze zovala ndi zakudya za tsiku lililonse , ’ ” koma osamupatsa zimene thupi lake likusoŵazo , kodi pali phindu lanji ? Mtima wawo uli pa kulemekeza Yehova , Ambuye Wamkulukulu . — Sal . N’zacisoni kuti anthu ambili masiku ano amadela nkhawa kwambili za tsogolo lao . Ndipo ambili amagwilitsa nchito moyo wao kufunafuna zinthu zosakhalitsa . Nditati ndiyese kuwaŵelenga , angakhale oculuka kwambili kuposa mcenga . ” Nthawi zina , mwamuna wakeyo sanali kukamba naye ndiponso anali kumuuza mau oipa cifukwa cakuti anali wa Mboni za Yehova . M’maiko aŵili onsewa , iwo satengako mbali m’ndale cifukwa ‘ sali mbali ya dzikoli , ’ ndipo akupitiliza kulalikila mwacangu ‘ uthenga wabwino wa mau opatulika . ’ — Yoh . 15 : 19 ; Mac . 8 : 4 . Mmene timagwilitsila nchito cikumbumtima cathu zimaonetsa kaya ubwenzi wathu ndi Yehova ndi wolimba kapena ai , ndiponso ngati tifuna kum’kondweletsa kapena ai . Pokumbukila pamene anali wacicepele , wadela wina anati : “ Kuŵelenga Baibulo yonse n’kumene kunan’thandiza kutsimikiza kuti Baibulo ni Maudi a Mulungu . Nimadziona kuti ndine wacabe - cabe . ” Malemba amaonetsa kuti anthu amene amacita zabwino n’colinga cakuti anthu ena awaone , sadzalandila mphoto iliyonse yocokela kwa Yehova . Tingaonetse bwanji kuti timacita zinthu mogwilizana ndi kudzipeleka kwathu ? Popeza Alexandra amasonkhana mu mpingo wa Mboni za Yehova wa cinenelo ca Cichainizi , anadzipeleka kuti amasulile zimene mnyamatayo anali kukamba . ( Ŵelengani Ezekieli 38 : 22 , 23 . ) Yesaya ndiye analemba zinthu zonsezi . Ndipo analembanso za lonjezo la Yehova lakuti adzasamalila anthu ake ndi kuwateteza akadzabwelela ku Yerusalemu . Kuti apume , munthu wopacikidwa anali kupuluputa . Abale ndi alongo ena amene anakwanilitsa colinga cawo cotumikila Yehova mu utumiki wanthawi zonse , pali pano akutumikila pa Beteli . Kodi Mumakhulupilila Kuti Muli ndi Coonadi ? Ngati nthawi zina mumalefulidwa polalikila m’gawo la anthu opanda cidwi , musadabwe nazo . Olo mtumwi Paulo , nthawi ina anamvelapo conco . Yesu anali kulola Mau a Mulungu kum’tsogolela pa zocita zake ndi pophunzitsa . Pamene Yesu anayamba utumiki wake padziko lapansi , iye anakamba kuti : “ Ndiyenela kukalengeza uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu kumizinda inanso , cifukwa ndi zimene anandituma kudzacita . ” Anati adzaciona ! Amuna na akazi anapatsidwa milandu yopandukila chechi na ziphunzitso zake , imene cilango cake cinali kuphedwa . ( Akolose 3 : 9 , 10 ) Conco , nthawi zina timalakwitsabe ngakhale kuti takhala Mboni kwa zaka zambili . M’malo mwake , iye anasiya zonse m’manja mwa Yehova . Conco , Mulungu afuna kuti mudzasangalale ndi moyo wabwino umene anafuna poyamba . Ine ndine Yehova . Popanda ine palibenso mpulumutsi wina . . . . Satana sangakwanitse kukakamiza anthu kucita zimene iwo safuna . “ Yehova akapanda kumanga nyumba , omanga nyumbayo amagwila nchito pacabe . ” — SAL . 127 : 1a . Gael anandionetsa zimene Baibulo limaphunzitsa m’ceniceni . M’bale wina amene akutumikila pa Beteli akakhala pa msonkhano wadela , nthawi zambili pulogilamu isanayambe amacezako na anthu amene akuyembekezela kubatizika . Ndine wokondwa cifukwa umoyo wanga tsopano , unasintha . 10 KUMASUKA MU UKAPOLO — KALE NA MASIKU ANO Iwo ali na mipata yambili yofutukulila utumiki wawo mwa kucita upainiya , kukatumikila kosoŵa , kugwila nchito ya cimango mogwilizana ndi Dipatimenti Yoona za Mapulani ndi Zomangamanga , komanso kufunsila kukaloŵa Sukulu ya Alengezi a Ufumu . Ambili a iwo amakhala acicepele . Yehova amadziŵa kuti timafuna kupezeka pamisonkhano ndipo amayamikila kuyesayesa kwathu Malangizo amene Yesu anapeleka mu ulaliki wake wa pa phili ni othandiza ngako popanga zosankha . Mu 1931 , Ophunzila Baibulo anasankha kudziŵika ndi dzina lakuti Mboni za Yehova . Kukhala pa ubwenzi wabwino ndi Yehova kudzatithandiza kupilila mayeselo . Rosa wa zaka 63 anakamba kuti , “ Jairo amakhala wokondwela . Kukhululuka kumatanthauza kuiŵalako zimene wina watilakwila na kucotsa mkwiyo , cakukhosi , komanso maganizo ofuna kubwezela . Amai anali kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova , koma sanafike pobatizidwa . Anthu ananyalanyaza zimene zinali kucitika mpaka cigumula cinafika n’kuwaseselatu onsewo . Mwacitsanzo , kodi m’mbuyomu munasintha zinthu zina kuti muyambe upainiya kapena kuti muonjezele utumiki wanu ? Mwacitsanzo , mvelani zimene Yoshiko wa ku Japan anakamba . Magetsi amathandiza kuti laiti iyake . N’cimodzi - modzi na kukoka mpweya . Komanso Shane , amene amagwila nchito yosamalila panyumba anakamba zofanana ndi zimenezi . Nanga n’ciani cimakupangitsani kukhulupilila kuti Yehova amamva mapemphelo anu ocokela pansi pa mtima ? Conco , ndi kusoŵa cikondi kusuliza mmene ena amasamalila acibale ao okalamba . Ganizilani zitsanzo zotsatilazi : Ndipo n’cifukwa ciani ? Baibulo limanenanso kuti tiyenela kupewa maganizo ofunitsitsa kulemela . Baibo imati : “ N’zosatheka kuti Mulungu aname . ” 10 : 8 - 12 ) Iye ayenela kuti anali kulimbikitsidwa akaganizila nthawi pamene anthu onse adzamasulidwa ku ucimo , imfa ndiponso ulamulilo wopondeleza . 25 : 5 , 6 . Kuti ateteze malile a dziko , maboma ambili amaikapo asilikali ndi zipangizo zina zamakono za citetezo . Ngakhale n’telo , ofalitsa anali kucititsa maphunzilo a Baibulo ambilimbili . Kodi mungam’thandize bwanji mwana wanu kuti akhutile na zimene amaphunzila m’Mau a Mulungu na kuzikhulupilila ? Mabuku ena akale aciyuda amakamba kuti akapolo ochulidwa palembali anali anthu a mitundu ina , amene anagwilizana ndi Abulahamu na Sara kulambila Yehova . Inu abale ndi alongo athu okalamba , dziŵani kuti enanso akhala akukumana ndi mavuto ngati anu . Conco tifunika kumukonda ndi kumumvela , cifukwa tikacimwa zimakhala ngati talephela kulipila nkhongole ya kumukonda popeza kucita chimo ndi kusakonda Mulungu . ” — 1 Yoh . 5 : 3 . Mwina timaona kuti anthu ocokela kumaiko ena ndi amanyazi ndipo amadzipatula . Khalani ndi cidalilo cakuti ana anu adzayamikila kwambili zimene mumacita powaphunzitsa . — Mat . Kuwonjezela apo , khalidwe lotayilila ndi laciwelewele zinali zofala mumzindawo . Iyi ni nthawi yanga yoyamba kukhala mumpingo wa cinenelo camanja . Anali kuyopa kuti anthu adzayamba kulemekeza kwambili iye m’malo mwa iwo . ( Onani ndime 7 , 8 ) Charles Darwin , m’buku lake lakuti The Descent of Man , anachula ziwalo zathupi zingapo kuti “ n’zosafunika kwenikweni . ” Mofanana ndi atate wake , Yehosafati analimbikitsa anthu kufuna - funa Yehova . Ndiyeno n’nawauza kuti , “ Mwakamba zoona . Komanso , kumbukilani kuti Mwana wokondeka wa Mulungu , amene anali kusangalala naye kwambili , anafa imfa yoŵaŵa . ( Miy . Tsiku lina mu October 1972 , mamembala 100 a m’gulu linalake la ndale ( Malawi Youth League ) anakonza zobwela kunyumba kwathu . Citsutso cimeneci cingasokoneze mgwilizano pakati pa otsatila ake na abululu awo . Pamene anafunsidwa kuti n’cifukwa ciani anayenda ulendo wautali conco , io anayankha kuti , ‘ Ndife ogwilizana ndi abale athu a ku Japan , ndipo tifunika kuwathandiza . ’ ” Apa n’kuti papita nthawi yocepa cabe kucokela pamene atsogoleli a Ciyudawo anasonkhezela anthu kupha Yesu . Masomphenya amenewa anaonetsa kuti Yesu anali wamoyo . Kudzicepetsa kumaphatikizapo kusadziika pamene suli , komanso kudziŵa bwino zimene sungakwanitse . ▪ Thandizani Kukongoletsa Paladaiso Wauzimu ( b ) N’ciani cidzacitikila anthu oipa amene sadzasintha ? Wamasalimo anakamba kuti Mulungu “ amatumiza mau ake padziko lapansi , ndipo mau akewo amathamanga kwambili . ” Panthawiyo , omasulila ambili anali asanaloŵe sukulu ya omasulila . Koma makolo ao akadwala , zimene zingabwele mwamsanga m’maganizo ao n’zakuti , ‘ Tiyeni tisiye utumiki kuti tikasamalile makolo athu . ’ 2 : 2 ) Mzimu umenewu umasonkhezela anthu kumangotsatila zimene anthu ambili amaona kuti ndiye zabwino . ( Yobu 2 : 3 ; 22 : 3 ; 27 : 5 ) Ifenso tingalimbane na nchito za Mdyelekezi mwa kulimbikitsa a m’banja lathu ndi Akhiristu anzathu . Iwo amagwila nchito yopanga mabuku kapena kuyang’anila nchito m’maiko amene nthambiyo imayang’anila . Lemba la Salimo 37 : 8 limati : “ Usapse mtima ndipo pewa kukwiya . ” ‘ Tsopano Ndinu Anthu a Mulungu ’ Zocitika zimene zinatsatilapo , zikuonetsa kuti Mulungu anamuthandiza kugwila bwino nchito yake . Pambuyo pa Sabata azimai anabwelela kumanda ndipo anapeza angelo amene anawauza za kuukitsidwa kwa Yesu . Malinga ndi kunena kwa Luka , azimai amenewa anali “ Mariya Mmagadala , Jowana ndi Mariya mai wa Yakobo . ” — Luka 23 : 55 – 24 : 10 . Popeza timatsatila malangizo a m’Baibo ndi a gulu , timalimbikitsa ukhondo , mtendele , na mgwilizano mumpingo . Koma pamene Yakobo ndi ana ake aamuna anasamukila ku Iguputo , io anatenga akazi ndi ana ao . — Gen . Tikacita zimenezo zimakhala zosavuta kukambilana momasuka . Anthu onse a Yehova amaona kuti Cikumbutso ndi cocitika capadela pacaka . ( Ŵelengani Akolose 3 : 9 , 10 , 12 . ) Koma kodi Yehova anamvela bwanji na zimene Asa anacita ? Kodi mungaonetse bwanji cifundo kwa anthu ena ? 2,858 N’ciani cinathandiza Yesu kupilila ? Nanga inuyo mungamutsanzile bwanji ? ( Aheb . 11 : 10 ) Abulahamu anali kuyembekezela nthawi imene adzakhala ndi malo okhazikika m’dziko lolamulidwa ndi Yehova . N’nali kufuna kuti azikhala womasuka kukamba nane ciliconse , kuphatikizapo mmene anali kumvelela mu mtima . ” Mu 2008 , anapita ku Ghana ndipo anatumikila kumeneko kwa zaka zoposa zitatu . Ndili ndi zaka 6 , banja lathu linasamukila ku Brazil kenako ku Ecuador cifukwa ca nchito ya atate . Conco , n’nacondelela Yehova m’pemphelo kuti anithandize . ” Kodi Mumacita Zinthu Mogwilizana ndi Cilungamo ca Yehova ? Ni liti pamene Petulo anathilila ndemanga pa lemba la Salimo 16 : 10 ? 32 : 8 . Kodi Mulungu anali kukamba ndi anthu m’Ciheberi cabe ? Zinali ngati kuti Mulungu wafufuta malile a maiko na cilaba cacikulu , ” anatelo Claire wa ku France . Monga Yesu , ifenso tiyenela kuyembekezela kuti utumiki wathu ungasinthe nthawi ndi nthawi . Kambili , izi zimacitika cifukwa ca zigamulo zimene zimapangidwa . Baibulo imakamba kuti , “ Mulungu amadana kwambili ndi aliyense wokonda ciwawa . ” Kunena zoona pali mavuto ena amene anthu sangakwanitse kuwathetsa . Athandizeni pa zinthu zina Comaliza , ngakhale anthu ena asiye coonadi ndi kusiya Yehova , tiyenela kukhala ndi ciyembekezo cakuti adzabwelelanso m’gulu la Mulungu . 3 , 4 . ( a ) N’cifukwa ciani Mose anacita mantha ? Mwina munayamba n’kale kuphunzila coonadi . Ndiyeno anthu onse adzakhala angwilo , ndipo Yehova adzawaona kukhala oyenelela kulandila moyo wosatha . Adani onse a anthu adzaonongedwa . Munthu wacikondi amakhululukila ena . Muzisankha mabwenzi amene ali ndi cikhulupililo colimba . ( b ) Fotokozani cocitika cimene cionetsa mmene Mulungu amatithandizila masiku ano . N’zinthu zinanso ziti zimene mungacite kuti muthandize anthu amene abwela mu mpingo mwanu ? Anthu ofika m’ma sauzande akuti anafa pamene anali kuoloka nyanja ya Atlantic . Sikuti ndalama zake zinawonjezeka . Cikhulupililo ca Petulo cinam’cititsa kuyenda pamadzi , cinthu cimene cinaoneka ngati cosatheka . N’zoona kuti pali acinyamata ena amene akugwilizana ndi mpingo omwe analeledwa ndi makolo amene si Mboni . M’Cigiriki , liwu lakuti ‘ kuyesetsa ’ kapena kuti kukalamila , limatanthauza kunyenyemphela kuti utenge cinacake pa malo amene sufikilapo . Koma nkhani imene tiyenela kutengamo mbali ndi yokhudza ulamulilo wa Yehova wa cilengedwe conse . M’pake kuti lemba la caka ca 2014 ndi Mateyo 6 : 10 , limene limati : “ Ufumu wanu ubwele . ” Kodi mudziŵako cipembedzo cililonse cimene cimakamba za uthenga wotelewu ? Olo kuti ukapolo waconco ni wosaloleka , ukupitila - pitila patsogolo . Ngakhale n’conco , zinthu zonse zimene anali nazo zinawonongeka . ( Mateyu 4 : 18 - 22 ) Nsomba zina zimene anthuwo anali kugwila m’nyanja imeneyo anali kuzikonzela ku mafakitale amene anali pafupi . Paulo anakumbutsa Akristu aciheberi kuti ayenela kulimbikitsana , kuonetsana cikondi , ndi kucitilana zinthu zabwino . Koma cimene ambili sadziŵa ni mgwilizano umene ulipo pakati pa cipilala na Baibo . Cipilala ca Tito cimacitila umboni woonetsa kuti maulosi a m’Baibo ni azoonadi . Umoyo wanga unali kuipilaipilabe . Mkaidiyo poyamba anali mkulu “ wopelekela cikho ” kwa mfumu . ( b ) N’ciani cimene ana anu angaphunzile ngati ndinu wodzicepetsa ndipo mumapewa kudzikonda ? N’zodziŵikilatu kuti magaŵano , tsankho , na cidani zidzaonjezeka m’dzikoli pamene mapeto akuyandikila . ( Agal . M’mbuyomo , madokota ananiuza kuti sinidzabeleka . Koma mu 1962 tinadabwa pamene n’nauzidwa kuti ndine woyembekezela . ( b ) Kodi zina mwa zifukwa zimene anakonzela buku la nyimbo latsopano n’ziti ? 69 : 9 ; Yoh . 2 : 17 ) Lelolino , palibe Nyumba ya Ufumu imene ingachedwe “ nyumba ya Yehova ” monga mmene analili kacisi wa ku Yerusalemu . “ Sindimvetsetsa mabuku oyela acipembedzo canga ca Cihindu . ( 2 Tim . 3 : 1 ) Mofanana ndi Yoswa , tingapambane ngati titsatila malangizo amene Yehova anam’patsa . 2 : 21 ) Ngati titsatila mapazi ake mosamala kwambili , tidzakhala “ otsimikiza kuti ” tidzapulumuka . Anthu ndi okondwela kwambili . ’ Tingagwilitsile nchito bwanji cidziŵitso cimene Yehova watipatsa kuti tionetse kuti timam’konda ? Woyang’anila hotela atasowa cocita anapempha alendowo ngati acinyamata angazipeleke kugwila nchito mu hotelayo , ndipo acinyamata ambili anadzipeleka mofunitsitsa . Yehova anatipatsa m’ndandanda wa ziyeneletso za akulu . Ngati mwauza mwana wanu kuti mudzamulanga akacita colakwika cina cake , muzisunga mau anu . Iwo amafika pojaila congo ca mamotokawo . Komanso amene amakhala kufupi na dzala , amajaila fungo loipa moti sadelanso nkhawa . Cimatithandiza kuonetsa kuti timafunitsitsa kuika patsogolo zofuna za ena Popeza posacedwa nidzakwanitsa zaka 80 , nimakondwela kuona anyamata amene n’nathandizila zaka zakumbuyo akutumikila pa maudindo amene n’nali kutumikila . Baibulo limati : “ Akazi azidzikongoletsa ndi zovala zoyenela , povala mwaulemu ndi mwanzelu , osati kudzikongoletsa ndi masitayilo omangila tsitsi , golide , ngale , kapena zovala zamtengo wapatali . Koma azidzikongoletsa mogwilizana ndi mmene akazi amene amati amalemekeza Mulungu amayenela kudzikongoletsela . Azidzikongoletsa ndi nchito zabwino . ” ( Luka 6 : 38 ) Tingasonyeze mtima wopatsa mwa kuitanila ena kunyumba kwathu kuti tidzadye nao cakudya ndi kucita nao zinthu zakuuzimu . 9 : 9 ; Luka 5 : 27 - 39 . Komabe , cofunika ndi mmene Mulungu anaonela zinthu , osati mmene anthu anali kuganizila kapena mmene mkazi wamasiye anali kudzionela . ( Salimo 143 : 8 ) Conco , tiyenela kudzifunsa kuti : Kodi zolinga zanga ndi mmene ndimagwilitsila nchito mphamvu ndi nthawi yanga zimaonetsa kuti ndimakondadi Yehova ? 30 : 21 . Zimenezo zidzatithandiza kudziŵa zimene tiyenela kukonza . John Milton , mzungu wina wolemba ndakatulo wa m’zaka za m’ma 1600 , amadziŵika cifukwa ca ndakakuto yake yakuti Paradise Lost ( Paradaiso Wotaika ) , yozikidwa pankhani ya m’buku ya Genesis yokhudza kucimwa kwa Adamu ndi kuthamangitsidwa kwake m’munda wa Edeni . Kuti tipambane , tifunika kudziŵa ceni - ceni cimene tikulimbanilana ndi adani athu . Sanafune kulemba zinthu zina zosafunika kwenikweni cifukwa cakuti anali kufuna kuonetsa kukoma kwa nyimbo yolembedwa mwa ndakatulo . Pakagwa za mwadzidzidzi , io amasinthila patsiku lina mlungu umodzi - modziwo . ( 2 Mbiri 16 : 9 ) Conco , Mulungu woona Yehova , amene ni wamphamvu kuposa Satana , adzakutetezani ngati mum’khulupilila . Koma mngelo anati : “ Ayi ! N’tafotokozela makolo anga nkhawa zanga , iwo ananilimbikitsa kuti nipite . Pofuna kutithandiza , Yesu anafunsa kuti : “ Ndani wa inu amene angatalikitse moyo wake pang’ono pokha mwa kuda nkhawa ? ” 22 ) Masiku anonso , kucita zimenezi kungakhale kofunika . Ngati Mkhristu wacita chimo lalikulu , amalandiwa udindo kapena mwayi wa mautumiki ena mu mpingo . Pamene Kaini anakwiya kwambili n’kufuna kupha Abele , Mulungu anam’patsa uphungu Kaini . Motelo , iye anayamikila Mulungu ndi Kristu cifukwa comusonyeza cifundo ndi kumpatsa utumiki ngakhale kuti kale anali munthu wocimwa . Yehova amatiteteza . Komabe , Yehova sanaletse zimenezi kucitika . Makolo acikhristu ali na udindo waukulu wolela ana awo “ m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake . ” Pa ndeu , ananilasa ndi mpeni ka 6 cakuti n’nacuca magazi kutsala pang’ono kufa . ” Kodi tingacite ciani kuti tizikonda kwambili zinthu za kuuzimu ? M’fanizo la anamwali 10 muli cenjezo lamphamvu . Izi zinawapatsa ciyembekezo . ( Eks . 32 : 21 - 24 ) Ndipo kodi mukanamva bwanji pamene Aroni ndi Miriamu anapandukila Mose cifukwa cokwatila mkazi wacikunja ? ( Num . Khalidwe langa linaonetselatu zimene zinali m’maganizo mwanga . Cinanso cimene Dipatimenti ya Magazini inali kucita ndi kutumiza magazini amene mipingo yaitanitsa . Njila imodzi imene tingacitile zimenezi ndi kuŵelenga lemba lililonse limene sanaligwile mau . Zoonadi , Yehova amakondwela ngako poona kuti tikuyesetsa na mtima wonse ‘ kubala zipatso zambili . ’ Mogwilizana ndi fanizolo , pamene mbuye anabwela , anapeza kuti kapolo amene anapatsidwa matalente asanu , anaonjezelanso ena asanu , ndipo kapolo amene anali ndi matalente aŵili , anaonjezelanso ena aŵili . “ Kugwilizana ndi anthu oipa kumaononga makhalidwe abwino . ” — 1 AKOR . Mu Salimo 16 , imene inalembewa na Davide , muli mau akuti : “ Simudzasiya moyo wanga m’Manda . Sikuti angakupatseni nchito ya ndalama zambili . Koma angakuthandizeni mwa kukukumbutsani mau a Mfumu Davide akuti : “ Ndinali mwana , ndipo tsopano ndakula , koma sindinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa , kapena ana ake akupemphapempha cakudya . ” ( Sal . Kodi Sayansi Imagwilizana ndi Baibulo ? 9 KODI MUDZIŴA ? Mwacitsanzo , pansi pa utsogoleli wacikanani , anthu anali kucita zinthu zonyansa , monga kugonana pa cibululu , kugonana amuna kapena akazi okha - okha , kugona nyama , kupeleka nsembe ana , ndi kulambila mafano . ( Lev . Tikamaphunzila za makhalidwe ake abwino ndi kuyesa kukhala “ otsanzila Mulungu , monga ana ake okondedwa , ndi kuyendabe m’cikondi , ” tidzakhala okonzeka kukana “ dama ndi conyansa camtundu uliwonse . ” ( Aef . Yakobo 1 : 14 , 15 Posakhalitsa nkhondo inafika poipa kwambili cifukwa palibe amene anaoneka kuti akugonja . Nthawi zina m’bale kapena mlongo akakonza zimene zaonongeka pa Nyumba ya Ufumu palibe amene amadziŵa . Jairo anabadwa ndi matenda ena ake a muubongo . Cilango cimene magulu onse aŵiliwa adzalandila cidzakhala cofanana . Iwo adzaonongedwa kothelatu . ( Maliko 3 : 14 ) Yesu analamula otsatila ake kuti : “ Conco pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzila anga . ” — Mateyu 28 : 18 - 20 . Kodi timadziŵa bwanji kuti nkhosazi zidzakhala padziko lapansi ? Buku limeneli likupezekanso pa www.jw.org M’madangawo munali mau a m’buku la Masalimo ocokela m’mabaibo asanu a Cilatini . M’bukuli munalinso chati ya maina audindo a Mulungu , kuphatikizapo zilembo zinayi za Ciheberi zoimila dzina la Mulungu . N’cifukwa ciani timagwila nchito imeneyi ? Zopeleka zathu zimathandizanso pa nchito yosamalila abale na alongo amene akutumikila ku likulu lathu na m’maofesi a nthambi osiyana - siyana pa dziko lonse . Kodi zimenezi zatheka bwanji ? Takhala tikugwilitsila nchito makompyuta ndiponso mapulogalamu ena a pakompyuta monga MEPS panchito yomasulila ( Multilanguage Electronic Publishing System ) . Ndisanafotokoze cifukwa cake , lekani ndikuuzeni za mbili yanga . Anacilitsanso anthu osaona ndi ofa ziwalo . Kapena n’cifukwa cakuti anali na “ cuma cambili ndi ulemelelo woculuka zedi ” ? Caka catha , tinatsogoza maphunzilo a Baibo oposa 10,000,000 . Ngakhale kuti makolo okalamba angafune kukhala okha ndi kumadzicitila zinthu , n’kofunika kuti io akambitsilane ndi ana za thandizo limene angafune pakabwela vuto . Komanso , akakumiza m’madzi si ndiye kuti akudzoza kuti ukhale mlaliki . ” Kodi mau athu angaonetse bwanji kuti ndife ozindikila ? Komatu cifunilo canu cicitike , osati canga . ” Anthufe ndi zinyama timafunika mpweya wa okisijini ndi cakudya , ndipo timatulutsa mpweya wa carbon dioxide ndi zinthu zina . Cilamulo cinateteza Aisiraeli mwauzimu powaletsa kukwatilana ndi anthu a cipembedzo conama . “ Mphatso iliyonse yabwino ndi yangwilo imacokela . . . kwa Atate . ” — YAK . Tiyeni tizikhala ofunitsitsa kusintha n’colinga cofuna kukondweletsa Yehova . — Sal . Olo zikhale conco , cilango cotelo cimaonetsa kuti Mulungu amam’konda munthuyo . Buku la Uthenga Wabwino la Maliko limakamba kuti Yosefe anali “ munthu wodziŵika wa m’Bungwe Lalikulu la Ayuda . ” Za sayansi zimasintha mofulumila kwambili , koma kodi zofunikila za anthu pa umoyo zasintha ? Kodi kuganizila zamtsogolo kunamulimbikitsa bwanji Enoki ? Akhristu ena amadziona kuti ni osayenelela kutumikila Yehova cifukwa anacita chimo lalikulu . KUKULA KWANGA : Ndinabadwa ndi kukulila m’komboni yaing’ono ku Rome imenenso munali ogwila nchito ovutika kwambili . Ngakhale munthuyo abwezedwe , amakhalabe woŵelengeledwa mlandu ‘ ku mpando wa ciweluzo wa Mulungu , ’ amene adziŵa bwino ngati kulapa kwake n’kwa zoona kapena ayi . — Aroma 14 : 10 - 12 ; onani Nsanja ya Mlonda ya Cizungu ya November 15 , 1979 , masa . ( Salimo 15 : 4 ) Popeza ndife okhulupilika kwa Yehova , tiyenela kusunga malonjezo athu . MULUNGU WAKUCITILANI ZAMBILI Mukaganizila zimene Mulungu wakucitilani ndi zimene wacitila anthu onse , mungavomeleze kuti iye wacita zambili . Yehova amaseŵenzetsa akulu acikhiristu kuti atiumbe , ndipo tifunika kumvela malangizo awo ( Onani ndime 12,13 ) Zoona zake n’zakuti anthu “ onse ndi ocimwa ndipo ndi opeleŵela pa ulemelelo wa Mulungu . ” — Aroma 3 : 23 . Conco , ngati sitikupezabe munthu wokwatilana naye , ndi bwino kuyembekeza ngakhale kuti tikufunitsitsa kukwatiwa . ” ( 1 Tim . Kulibe boma la anthu limene lingathetseletu nkhanza , kupanda cilungamo kapena matenda . N’cifukwa ciani nthawi zina akulu amanyalanyaza kuphunzitsa ena ? Kodi mumalakalaka Mulungu atakonza zinthu ? Tsopano m’dzikoli muli anthu ambili odzikonda , okonda ndalama , na zosangalatsa . M’masomphenyawo , anauzidwa kuti : “ Wolokelani ku Makedoniya kuno . ” A Willie anauza amayi kuti : “ Atate anu ali ku helo ! ” Monga mmene Salimo 119 ionetsela , kodi Mau a Mulungu anam’thandiza bwanji wolemba salimo ? N’zinthu ziti zimene anthu sangakwanitse kucita ? Pali zinthu ziŵili zofunika zimene mungacite : Muzikonzekela bwino , komanso musaleke kuuzako ena zimene munaphunzila . Baibulo limati : “ Kristu ndiye kutha kwa Cilamulo . ” Aisiraeli anali kutsogoleledwa ndi Gidiyoni . 10 : 18 - 20 ) Olamulila aumunthu ndi akuluakulu a boma sali kanthu powayelekezela ndi Yehova . Anthu amakhulupilila kuti munthu amangomasuka ku moyo wobadwanso kukhala cinthu cina ngati akhala ndi moyo wabwino ndiponso cidziŵitso capadela . Cimeneci ndi citsanzo cabwino kwambili kwa acinyamata masiku ano . Muyenela ‘ kulemekeza atate ndi amai anu ’ ngakhale kuti io si Mboni . ( Eks . 20 : 12 ; Miy . Ndipo mofanana ndi Eliya , mwina mwacita zambili mu utumiki wanu kwa Yehova kuposa mmene mumaonela . Kapena mwathandiza ena mumpingo popanda inu kudziŵa . Vidiyo yakuti Cikondi Ceniceni inabwela panthawi yake . Jan . Kudzicepetsa kumatithandiza kumvela mfundo yofunika kwambili imene Yesu anakamba . Akulu , kumbukilani kuti mphunzitsi wabwino sayenela kukonda cabe nchito yophunzitsa koma ayenelanso kukonda wophunzila . Kodi ana ena amacita ciani kuti azilemekeza ndi kusamalila makolo ao amene akhala kutali ndi io ? Koma iye sanafunike kulowa m’malo Eliya nthawi yomweyo . A Zulu : Zoona zake n’zakuti , Danieli sanadziŵe tanthauzo la maulosiwo cifukwa cakuti nthawi ya Mulungu inali isanakwane yakuti anthu azindikile tanthauzo la maulosi amenewo . M’cakaci m’pamene masiku otsiliza , kapena kuti nthawi ya mapeto a dziko lino anayamba . Pamene tikuphunzila na kusinkha - sinkha Mau a Mulungu , tizicita zimenezo tili na mtima wofunitsitsa kukondweletsa Yehova na kumvela malamulo ake . ( Sal . Conco kwa anthu ambili , imfa ni sitepi yofunika kwambili yoloŵela ku moyo winanso , ndipo amaiona kuti n’cifunilo ca Mulungu . Ndipo Simone anati : “ Ni mwayi waukulu ngako kutumikila kuno ku Myanmar . Ena mwa anthu amenewa amacita zoipa moonetsela . Palibe munthu amene angakuyankhileni mafunso amenewa . Ndipo Yehova amafuna kuti muziwaphunzitsa ndi kuwalangiza . M’nthawi ya Yesu , atsogoleli ena acipembedzo anali na mtima wofuna kukhala odziŵika kwambili kwa ena . Pamene John anafika , mkazi wa m’baleyo , amenenso anali wa Mboni za Yehova , analandila kalatayo . Lekani ndikuuzeni mbili yanga . 14 Madalitso “ m’Nthawi Yabwino ndi m’Nthawi Yovuta ” Ngati sitim’pempha kuti atikhululukile , zingafanane ndi munthu amene akukana kusamba m’manja kuti acotse dothi . Kodi iye akanalimba mtima kumanga kacisiyo ? Yendani mmenemu . ” ​ — YESAYA 30 : 21 . 9 , 10 . ( a ) Kodi ndi liti pamene Kristu anamangilila lupanga m’ciuno mwake ? Ndiyeno tsiku lina a Mboni anafika panyumba n’kundipempha kuphunzila nao Baibulo ndipo ndinavomela kuphunzila nao . ” — Anju , Nepal . ( b ) Kodi ndi cinthu comaliza citi cimene Yesu adzacita monga Mfumu Mesiya ? Nanga zimenezo zidzakhudza bwanji colinga ca Yehova ? Ndiponso , kugwila nao nchitoyi kumalimbitsa cikondi ndi m’gwilizano . ” Mungaŵelenge naye lemba la Tito 2 : 10 ndi kumufotokozela kuti Nyumba ya Ufumu ifunika kukhala yaukhondo n’colinga cakuti ‘ ikometsele ciphunzitso ca Mpulumutsi wathu Mulungu . ’ Pamene Simoni anadziŵa kuti maganizo ake anali olakwika , anapempha atumwiwo kuti amupemphelele kuti athetse maganizo akewo . — Machitidwe 8 : 18 - 24 . Funso limeneli n’lofunika kwambili , makamaka kwa aja amene anataikilidwa anzao a m’cikwati . Kutsamilitsa mutu wake pa mapilo kungathandize kuti wodwala asamasanze . ( 1 Yoh . 4 : 8 ) Tifunika kupewa kukhala na maganizo akuti , “ Ningafunike kuwakonda abale anga cifukwa ni lamulo ngakhale sinikondwela nawo . ” Cina , Mulungu anam’sintha dzina . Pamene munthu wadzipeleka kwa Yehova , amamuuza kuti : “ Ndakupatsani moyo wanga , ndipo ndine wanu . ” Koma Sara , amene anali mfulu , anali kuimila mkazi wa Mulungu , limene ndi mbali yakumwamba ya gulu lake . N’zoona kuti angacotse mayeselowo ngati afuna . N’nali kugona pa mphasa . Bafa yosambila sinali kanyumba kochingika bwino ayi . Ndiyeno , dzifunseni kuti : ‘ Kodi nimatsatila malangizo amenewa mu umoyo wanga ? Mwacitsanzo , kodi mumakhulupililadi kuti tikukhala m’masiku otsiliza ? 6 : 20 ; 7 : 1 - 3 ) Ndiponso , Paulo anayelekezela mneneli Yesaya ndi ana ake aamuna kuti anali kuimila Yesu ndi otsatila ake odzozedwa . ( Aheb . Kucokela nthawiyo , Yehova wandiphunzitsa , ndipo tsopano ndimacita zinthu mosamala polalikila ndi kuphunzitsa ena . — Akol . Kodi munthu amene akuvutika ndi maganizo olakwika angakhale bwanji ndi maganizo oyenela ? Anakambanso kuti : “ Kuphika cakudya kunali kutenga nthawi yaitali kuwilikiza ka 10 ndi nthawi imene tinali kutenga pophika cakudya kwathu . Timagwila nchito imeneyi pa mlingo waukulu cifukwa timalalikila anthu a mitundu yonse ndi zinenelo zonse . Pambuyo pake , Eliya anapemphela kwa Yehova , ndipo Mulungu anamuyankha mwa kutumiza moto kucokela kumwamba . Ngati nyumba iliyonse inacita kumangiwa na winawake , kuli bwanji zamoyo ? COLINGA : Kupanga makonzedwe ovomelezeka a Yesu , amene ndi mbali yoyamba ya “ mbeu ” ya mkazi . Iye adzakhala mfumu ndi wansembe kwamuyaya Ŵelengani maulosi a m’Baibulo amene anakwanilitsidwa kale . Kumbukilani kuti iye anacita cigololo na Bati - seba , komanso anafuna kupha munthu waumbombo Nabala ndi banja lake . Amuna onse amene anasankhidwa , anali na maina a Cigiriki . Ndinaganiza kuti mwa kucita zimenezo ndizadziŵa coonadi . Tikatelo , anthu adzatidziŵa msanga kuti ndife Mboni za Yehova . 18 Cocitika Cosaiŵalika pa Utumiki Wanga wa Ufumu Abale ena amatsutsana ndi anthu pa intaneti pa nkhani za Mulungu , ndipo izi zawonjezela citonzo pa dzina la Yehova . Tikapeza covala cabwino komanso coyenelela , Akhiristu anzathu adzayamikila kwambili , ndipo sitidzacita naco manyazi . 15 : 1 - 4 ) Ndiyeno , pambuyo pa miyezi pafupifupi itatu , Yehova anacita pangano ndi Aisiraeli pa Phili la Sinai . Iye anawalonjeza kuti : “ Ngati mudzalabadiladi mau anga ndi kusunga pangano langa , pamenepo mudzakhaladi cuma canga capadela pakati pa anthu ena onse , . . . ndi mtundu wanga woyela . ” — Eks . Patapita nthawi yocepa , n’naitanidwa kuti nikatumikile ku Beteli , ndipo n’nayamba kuseŵenzela ku Watchtower Farm , m’dela la Staten Island , ku New York . Kodi mungasintheko zinthu zina n’colinga cakuti mukhale na nthawi yoceleza ena kapena yokaceza kwa Akhristu amene akuitanilani ku nyumba kwawo ? Posonyeza kuyamikila makonzedwe a kacisi wauzimu , timatamanda Yehova ndi kumukweza mwa kulengeza dzina lake cifukwa anatipatsa dipo mwa cifundo cake . Amangofuna kuti zawo ziziwayendela . Iye anadziŵa kuti khandalo likadzakula lidzakhala Mesiya wolonjezedwa . ( Aroma 2 : 14 , 15 ) Anthu ambili amakonda zinthu zaukhondo ndi zokongola . Iwo anakambanso kuti sanamuonepo atakwiya . ( Onani ndime 15 , 16 ) Ponena za banjali , akuluwo anati : “ Iwo ni apainiya okhala na umoyo wosalila zambili , ndipo akupeleka citsanzo cabwino pankhani yofuna - funa Ufumu coyamba . ” — Luka 12 : 31 . Iye anati : “ Nditakumbukila za cinyengo cimene cinali m’chalichi canga cakale , ndinasankha kutula pansi maudindo amenewa . Kodi Yesu anatanthauzanji pokamba kuti tizikonda Mulungu ndi ‘ mtima wathu wonse ’ ? Yehova anali kuniphunzitsa kupitila m’gulu lake . ” Mudzakasangalala kwambili kumvela Mtsogoleli wanu Yesu , akukuuzani kuti : “ Pa mlingo umene munacitila zimenezo mmodzi wa abale anga aang’ono awa , munacitila ine amene . ” — Mat . Anthu ambili amaika moyo wawo paciswe pofuna kusamukila ku maiko olemela . Pamene acinyamatawo anaona m’mafaelowo , anapezamo makalata ambili amene abale m’madela osiyanasiyana m’dziko lonse la Malawi anandilembela . ( b ) N’cifukwa ciani Mose anamvela malangizo a Mulungu ? Cina cimene cinathandiza anthu akale kukhalabe na cikhulupililo colimba , ni pemphelo . Anakamba kuti Akristuwo anali ndi mzimu wopilila . Mbali imeneyi ya kuleza mtima yafotokozedwa bwino pa Yakobo 5 : 7 , 8 . Yehova , Mlengi wa malekezelo a dziko lapansi , ndiye Mulungu mpaka kalekale . ” Iye analemba kuti : “ Koma Ambuye anaima pafupi ndi ine ndi kundipatsa mphamvu . ” Kodi abale amenewa angaphunzitse bwanji ena m’mipingo ? Taro anakamba kuti : “ Iwo anakwiya kwambili cakuti kwa zaka zambili , anali kundiletsa kupita kukawacezela kunyumba . Kenako tinaikidwa kukhala apainiya apadela , ndipo pambuyo pake anatitumiza kukatumikila m’dela . Kuonjezela pamenepa , iye “ sanaticitile mogwilizana ndi macimo athu , ” koma mwacifundo amatikhululukila tikalapa . — Salimo 103 : 10 , 14 . ( 1 Timoteyo 1 : 17 ) Izi zitanthauza kuti Mulungu wakhalapo kuyambila kalekale kuposa pamene maganizo athu angafike tikamaganizila za m’mbuyo . KUPATSA . N’ciani cingatithandize kupanga zosankha mwanzelu ngati Baibulo silikamba mwacindunji zimene tiyenela kucita ? Cikondi ndi cifundo ca Yehova Mulungu zakhudza kwambili umoyo wanga . Kwa munthu wosaphunzila , liu lakuti הנפשׁ ( han·ne’phesh ) lingaoneke losiyana kwambili ndi liu lakuti נפשׁ ( ne’phesh ) . Mmodzi wa “ mafumu ” amene Paulo anaima pamaso pake anali Nero , Mfumu ya Roma . Komanso , kukonda Mulungu na coonadi sikuli monga coloŵa cimene munthu amalandila kwa makolo ake . ( Aheb . 3 : 12 , 13 ) Koma kodi zimenezi zitanthauza kuti anthu otelo basi anathimbilila sangasinthe ? Tili ndi nchito yolengeza “ uthenga wabwino ” kwa anthu padziko lonse lapansi mapeto asanafike . Kodi nimakondwela maningi nikakhala kuti sinili pamodzi na mwamuna kapena mkazi wanga ? Panthawiyo , Yehova Mulungu , “ Ambuye woona ” pamodzi na Yesu Khiristu , “ mthenga wa pangano , ” anabwela ku kacisi wauzimu kudzayendela otumikila m’kacisiyo . Iye anauzanso Ahabu uthenga waciweluzo wocokela kwa Mulungu . Izi ni zocepa cabe mwa zinthu zokondweletsa zimene anthu amene adzipezela mabwenzi kumwamba adzasangalala nazo . Hans anati : “ Tsiku lina tinamvetsela nkhani pa msonkhano wacigawo imene inafotokoza kuti pamene Mfumu Davide anauzidwa kuti sayenela kumanga kacisi , anavomeleza ndipo anasintha colinga cake . Oksana , Aleksey , ndi Yury Popeza kuti khalidwe laciwelewele lafala masiku ano , amuna ndi akazi afunika citsogozo ndi citetezo ca Yehova kuti akwanitse kuteteza ukwati wao . Iye analimbikitsa anthu kutumikila Yehova . Tikamakumbukila kuti Mulungu amaona zili m’maganizo mwathu na zocita zathu , tidzafuna kukhala oyela kuti tim’kondweletse . — Ŵelengani Mateyu 5 : 27 , 28 ; Aheberi 4 : 13 . Ngati munayamba kale upainiya , mwina mungafunsile kuti muloŵe Sukulu ya Alengezi a Ufumu . Ine na mkazi wanga tinazindikila kuti Mboni zimacita zinthu mosiyana ndi ena . M’pemphelo lina , Yesu anachula Yehova kuti “ Atate Woyela . ” Cikondi ca a ga’pe cozikidwa pa mfundo zabwino ndiye cikondi capamwamba kwambili . Koma Toñi anapepesanso na kuuza mzimayiyo kuti anali kumvetsa mavuto amene anali kukumana nawo . Cinthu cimene ndimakonda kwambili ndi kusonkhana . ” Mauwa aonetsa kuti zimene munthu amalakalaka zingacititse kuti ayamikile mphatso kapena ayi . Ganizilaninso zimene angadzakufunseni ponena za umoyo wanu m’masiku otsiliza . 138 : 6 . Colinga cake ca poyamba cinali cakuti anthu akhale kwamuyaya pano padziko lapansi monga ana ake omvela . Agaluwo atafika pafupi , anaima na kuyamba kukweteza micila , ndipo kenako anacoka . Mphatso imeneyi ‘ ingakulimbikitseni m’njila yosalephela ndiponso ingakupatseni ciyembekezo cabwino . . . kukulimbikitsani muntchito yabwino iliyonse ndiponso m’mau . ’ — 2 Atesalonika 2 : 16 , 17 . Timaphunzitsidwa ndi Yehova . Anapeza kuti ku delalo kuli mpingo wokhala ndi ofalitsa 69 , apainiya a nthawi zonse 13 , ndipo onse anali kusonkhanila m’Nyumba ya Ufumu yatsopano . NYIMBO : 57 , 48 “ Masiku otsiliza adzakhala nthawi yapadela komanso yovuta . ” Ndithudi , unali mwai waukulu kukhala mai wa munthu wa mkulu amene anakhalapo padziko lapansi . — Mat . Ayuda ena anafika polemela . Mwacitsanzo , tingakambe kuti , “ Taonani zimene Mlengi anakamba pankhaniyi . ” Nthawi zambili makhalidwe athu abwino monga ciyelo ndi mtendele ndi amene amacititsa anthu kuyandikila Mulungu ndi Kristu ndiponso kubwela m’gulu la Yehova . Anthu odzicepetsa angadziŵe Yehova ndi kukhala naye paubale wathithithi kokha kupyolela mwa Yesu . Choong Keon anati : “ Tinaganiza kuti ndi bwino kuleka ‘ kungoyang’ana , ’ koma kuyamba ‘ kubzala ndi kukolola . ’ ” Kodi “ cofufumitsa ” cimene Yesu anauza ophunzila ake kuti afunika kupewa cinali ciani ? ( 1 Mafumu 9 : 4 ) Mukanakhalapo nthawi imeneyo , kodi mukanamvela bwanji ndi zimene Davide anacita ? Ganizilani izi : Panthawiyo wamasalimo anali kuziona nyenyezi , koma sanali kudziŵa kuti zilipo zingati . N’nayamikila Yehova cifukwa conipatsa mnzanga amene amanifunila zabwino . ” Pakona ya kum’mwela ca kum’mawa kwa kacisi , panali denga lafulati limene linali lalitali kwambili . Makolo okalamba angadwale cifukwa ca maganizo . ( Aefeso 2 : 2 ) Kuti tipeweletu kutenga mbali m’ndale , sitiyenela kuona kuti anthu ena a ndale ndi abwino kuposa ena . Kodi taphunzila ciani pambuyo popenda maumboni atatu osonyeza kuti tikukhala m’masiku otsiliza ? Ndipo izi zilidi conco m’maiko ambili . ( Oweruza 11 : 35 ) Yehova analandila nsembe yamtengo wapatali ya Yefita ndipo anam’dalitsa . Mayankho anu pa mafunso amenewa adzaonetsa ngati ubwenzi wanu ndi Yehova ndi wolimba . Nyembazi amaziyanika pa dzuwa kuti ziume . Nthawi zambili , tuakacisi tumenetu tumakhala ndi mafano ndiponso zinthu zopatulika zacipembedzo , zimene io amakhulupilila kuti n’zogwilizana ndi zozizwitsa , maloto , kapena mizimu ya anthu akufa . N’nadabwa kuti M’bale Hughes anali kumwetulila pamene anali kuniuza zimenezi . Malembawo aonetsa kuti Mulungu ndi “ Mfumu yamuyaya , ” monga mmene mtumwi Paulo anafotokozela . Iye anakana kwa mutu wa galu , uku maso ake ali tong’o . Ndipo Yehova anaonetsetsa kuti nkhaniyi yalembedwa ‘ kuti itilangize ndi kutipatsa ciyembekezo cifukwa malemba amatithandiza kupilila ndiponso amatilimbikitsa . ’ ( a ) Pambuyo pa Cigumula , kodi n’kuti kumene anthu anayambila kupandukila Yehova ? Modzikuza ananyalanyaza uphungu umene Yehova anamupatsa ndipo anapha m’bale wake . — Gen . “ [ Yesu ] anawauza kuti : ‘ . . . Onetsani cifundo kwa ena mwa kuwathandiza pamene afuna thandizo ( Onani palagilafu 12 ) Baibulo limakamba kuti : “ Khulupilila Yehova ndi mtima wako wonse , ndipo usadalile luso lako lomvetsa zinthu . Joshua , amene ali ndi zaka 25 , anati : “ Kudzipezela zinthu zofunikila pa umoyo n’kofunika . Mungacite ciani kuti muwonjezele kuwala kwa coonadi ca m’Baibo m’dela lanu ? Liu la Cigiriki limene linamasulidwa kuti “ onenela anzawo zoipa , ” kapena kuti “ woneneza ” ni di·aʹbo·los . Ndinamvapo za Baibulo koyamba ndili ndi zaka 17 . Amuna anali kukwatila ndipo akazi anali kukwatiwa , kufikila tsiku limene Nowa analoŵa m’cingalawa . 3 : 11 , 12 ) Pocita izi , tifunika kukumbukila kuti nafenso ndife opanda ungwilo ndipo tingathe kulakwila anzathu . Mwacitsanzo , ataona anthu ambili akumulondola kuti amve mau ake , anapatula nthawi yokhala nao ndi kuwaphunzitsa . Coyamba , Yehova amakutsimikizilani kuti : “ Ndikulimbitsa . Miyala ina ya dayamondi amaigulitsa madola mamiliyoni ambilimbili . Ku mbali yathu tili na Yehova , Yesu , na angelo okhulupilika . ( Miy . 14 : 29 ) “ Amayenda panjila yabwino , ” kutanthauza kuti amapanga zosankha zabwino paumoyo wake . ( Miy . Patapita miyezi 9 ndinabatizidwa . 9 : 22 ) Paulo anafotokozanso kuti nsembe zanyama , ngakhale kuti zinali kugwila nchito pamlingo wocepa , zinali kungokumbutsa Aisiraeli kuti anali ocimwa , ndi kuti anafunikila nsembe yoposa yanyama kuti icotseletu macimo ao . 31 : 28 ) Kucita umutu mwanjila imeneyi kudzacititsa kuti akazi ao adziwakonda ndi kuwalemekeza , ndipo Mulungu adzadalitsa banja lao . Nanga bwanji ngati panthawiyo tidzapemphedwa kugwila nchito inayake imene siitisangalatsa ? Dzina la Mulungu : Potengela mwambo wa Ayuda , omasulila Baibulo ambili anaganiza zocotsa dzina la Mulungu m’Malemba . Kodi Yesu Ananyoza Pokamba Fanizo la “ Tiagalu ” ? Mwacitsanzo , mwana wamng’ono sangamvetsetse kuopsa kogwilizana na anthu oipa . Kuti mudziŵe zambili pankhani ya zizindikilo za masiku otsiliza , ŵelengani nkhani 9 yakuti ; “ Kodi Tili mu ‘ Masiku Otsiliza ’ ? ” Pofuna kutithandiza kuti tikhalebe na cikhulupililo colimba , Yehova mokoma mtima watipatsa mau ake Baibo . Panalinso Mboni za Yehova za m’delalo zimene zinabwela kudzacingamila M’bale Rutherford , amene anabwela ku msonkhano waukulu wa masiku atatu . Ndipo pamene dziko liipilaipila , anthu a Yehova apitiliza kulimbitsa cikhulupililo cao , kukhala acangu , ndi kukondana . Iwo anafunika ‘ kusankha moyo . ’ 9 , 10 . ( a ) N’cifukwa ciani Yehova amatiuza za iye ? Anali Rabeka . N’nabadwa mu 1928 , ndipo ndine wotsilizila pa ana 6 . Ndiponso zofuna za anthu ofunika cisamalilo zimasiyana . Nthawi zina kholo lokalamba lingakambe mau opweteka kapena kuonetsa kusayamikila . Tiyenela kupemphela ndi kuganizila mozama zimene taphunzila zokhudza Yehova , zimene amakonda , zimene amadana nazo , ndi zimene anacita m’mbuyomu Iye sanakwanitse kukambilana ndi anthu nkhani za m’Baibo . Conco , anauza abale ena a pa Beteli kuti , “ Ngati pali dziko limene sinifuna kukakhako mu umoyo wanga , ni Portugal . ” Kupilila Mwacitsanzo , m’bale wina amene mwana wake anadzipha anafunsa kuti : ‘ Kodi Yehova anadziŵilatu kuti ine na mkazi wanga tidzakwanitsa kupilila imfa ya mwana wathu ? Abulahamu anaonetsa cikhulupililo ndipo anali wokonzeka kupeleka Isaki monga nsembe Atate wathu Yehova watipatsa ufulu wodzisankhila zocita . Kodi Natani anacita ciani ? Kodi tingafotokoze nkhani ya pa Lemba limene dzina lathu lakuti Mboni za Yehova licokela ? Iwo ndi munthu woona mtima amene wakhala akugwila nchito mwamphamvu nthawi zonse , ndipo nchito imene agwila kwa nthawi yaitali ndi ya ukalipentala . Koma kodi zitanthauza kuti iye wakhala na nzelu ? Kodi Mukukalamila Udindo ? 9 / 15 Conco , aliyense afunika kusankha kuti wolamulila wabwino ndi uti pakati pa Mulungu ndi Satana . Fotokozani mmene tingagwilitsile nchito Yesaya 14 : 7 mu ulaliki . 7 : 10 ) Zolengedwa zauzimu za Mulungu zimachedwa kuti “ makamu ” a Yehova ndipo ndi zadongosolo . — Sal . Patapita zaka 5 , anatipempha kuti tibwelelenso kuno ku Japan , kumene tikupitiliza kutumikila m’dela . N’tabwelela ku Germany , n’naganiza zakuti nizicita zofananazo . Nkhani zimenezi zinathandiza mlongo wina dzina lake April kuyamba kuphunzila Baibulo ndi anthu atatu amene amagwila nao nchito . Koma acibale anga sanapitilize kuphunzila Baibulo panthawiyo . Abale ambili angaone kuti ayembekezela kwa nthawi yaitali asanaikidwe pa udindo . Mpanda wa Yerusalemu unamangidwanso mu 455 B.C.E . , motsogozedwa ndi Nehemiya . Takulandilani . ” Motelo anaganiza zofufuza kuti aone ngati aliyense m’bwatolo anali ndi khadi la cipani . ( Gen . 14 : 14 - 16 ) M’nthawi ya Mfumu Davide anthu amene anali kuimba pa nyumba ya Mulungu ‘ anaphunzitsidwa kuimba ’ nyimbo zotamanda Yehova . Tili ndi moyo cifukwa ca io , ndipo anatipulumutsa ku ucimo ndi imfa . ( Mat . 6 : 28 - 30 , 33 ) Ndithudi , Atate wathu wakumwamba Yehova , amakukondani inu makolo ndi ana anu , ndipo amafuna kuti zinthu zizikuyendelani bwino . Iye ayenela kuti anaphunzila kacitidwe kawo ka zinthu kwa nthawi yaitali akalibe kuwakopa kuti akhale ku mbali yake . Baibulo limakamba kuti : “ [ Mose ] anatenga buku la pangano ndi kuŵelengela anthuwo kuti amve . M’pemphelo lake Mfumu Davide anafunsa kuti : “ Kodi mudzandiiŵala kufikila liti ? Conco , tisanyengedwe ndi mabodza a Satana . Nkhani ino idzatithandiza kukhala na maganizo oyenela , amene Yehova Mulungu amavomeleza , pa nkhani yofuna kukhala wodziŵika kwa ena . Cakudya cikusoŵabe ngakhale kuti kuyambila m’caka ca 1914 anthu apita patsogolo pa zacuma ndi zasayansi . 22 : 3 ) Ngati mwakumana naco ciyeso , pemphani Yehova kuti akupatseni nzelu ndi kukuthandizani kukhala odziletsa . Njila yacitatu , ni kutengela citsanzo ca Yehova coyang’ana zabwino mwa ena . Nanga ndi zinthu ziti zimene akazi okhulupilika akale anacita ? Kuonjezela apo , anthu ena amakhala ndi nkhawa zaumwini ndipo amadzifunsa kuti , ‘ Kodi ndidzakhala ndi khansa ya pakhungu ? ’ Koma ngakhale masiku ano , timakwanitsa kum’lambila cifukwa ca mphatso ya dipo imene watipatsa . Mfumu Davide waitana akalonga ake onse , nduna za mfumu , ndi amuna olemekezeka . ( Yelekezelani ndi Yohane 5 : 20 . ) Tikukhala ‘ m’masiku otsiliza , ’ ndipo posacedwapa tikumana ndi cisautso cacikulu cimene sicinacitikepo n’kale lonse . ( Yakobo 1 : 17 ) N’zacionekele kuti lembali likamba za kuolowa manja kwa Atate wathu wakumwamba , Yehova Mulungu . Vuto ndi lakuti matembenuzidwe amenewa alibe maziko . 19 : 13 ) Mosiyanako , anthu a Mulungu akale anaona mmene atsogoleli awo okhulupilika analimbitsila ciyelo cauzimu , cakuthupi ndi makhalidwe abwino . Tiyenela kutengela Yesu mwa kuthandiza anthu onse kudziŵa zinthu zabwino zimene Mulungu watilonjeza . DON , mmodzi wa Mboni za Yehova ku Canada , amayesetsa kulalikila anthu ovutika amene amakhala m’miseu . Izi zinam’thandiza kuti vuto lake lisafike poipilatu . Nanga tingakhale nalo bwanji khalidwe laumulungu limeneli ? Pamene iye anali m’ndende ku Iguputo , kodi anali kudziŵa kuti m’tsogolo adzaikidwa kukhala waciŵili kwa mfumu ya dzikolo ? Nanga kodi anali kudziŵa kuti Yehova adzamuseŵenzetsa kupulumutsa acibale ake ku njala imene inacitika ? ( Gen . Kodi Yehova anakhala Mpatsi Wamkulu kwa Abulahamu ndi Isaki m’njila yotani ? 16 , 17 . ( a ) Pelekani fanizo losonyeza zimene kudzipeleka kumatanthauza . ( b ) Kodi munthu amene wadzipeleka kwa Mulungu amakhala akumuuza ciani kwenikweni ? Ndipo m’pamene umaona bwino kuti Yehova akukusamalila kwambili . ” Komabe , makolo anzelu amacita zinthu molimba mtima ndipo amakhulupilila malonjezo a Yehova . Nanga n’ciani cidzacitika kwa anthu ambili - mbili amene anafa ndipo sanapite kumwamba ? Yelekezani kuti mukuona Yosefe akuyang’ana kuthambo lakumadzulo kumene dzuŵa linali pafupi kuloŵa , ndipo akuganizila mmene zinthu zafikila poipa kwambili pa umoyo wake . A Inoki : Zikomo kwambili . Ku mbali ina , “ munthu wauzimu amafufuza zinthu zonse , ” ndipo amakhala na “ maganizo a Khristu . ” Koma malinga n’zimene Alexei na Huabi anapeza , Baibo imayankha mafunso ofunika kwambili akuti “ n’cifukwa ciani , ” monga akuti : N’cifukwa ciani zinthu zinalengewa ? Pamene m’bale wina ku Tulun ananiuza kuti kukubwela mlongo , n’napita ku sitesheni na njinga yanga kuti nikam’landile . Kodi Mulungu wathandiza bwanji anthu kuti amve Mau ake olo kuti zinenelo zakhala zikusintha ? Akazi anali kupela ufa wophikila mkate ndi manja , ndipo imeneyi inali imodzi mwa nchito zimene anali kugwila m’mamaŵa . Pampingo winanso iye ndi amene anali kukamba nkhani zambili za mu Msonkhano wa Nchito . Anali kucititsanso Sukulu ya Ulaliki , Phunzilo la Nsanja ya Mlonda ndi kutsogoza Maphunzilo 5 a Buku a Mpingo . Ni malangizo anji amene mtumwi Paulo analembela Akhristu anzake ? Atauzidwa kuti ndi Isaki , iye anatenga nsalu yophimba kumutu n’kudziphimba nayo . Conco , caka cisanathe amayi anavomela kuti nicoke pa sukulupo . Komabe , Baibulo limatitsimikizila kuti Mulungu amamva mapemphelo . 11 : 29 ) Pambuyo pake , “ Aisiraeli anayamba kuopa Yehova ndi kukhulupilila Yehova ndi mtumiki wake Mose . ” — Eks . M’bale George Gangas , amene anatumikila m’Bungwe lolamulila kwa zaka zoposa 22 , anati : “ Ndimasangalala kwambili kusonkhana pamodzi ndi abale cifukwa ndimalimbikitsidwa . ( b ) Ngati tilalikila , ndiye kuti tikuthandiza bwanji kapolo wokhulupilika na Yesu ? Anthu onse anali kuyang’ana ku nyanja . ( Yesaya 26 : 20 ) ‘ Zipinda zamkati ’ zimenezi zingatanthauze mipingo yathu . Ndipo pali maumboni amphamvu otsimikizila zimenezi . Ufumu wa Mulungu wokha ndiwo ungacotse mavuto amenewa . 4 : 18 ) Conco , muziphunzila Mau a Mulungu mozama . Tinakhala kumeneko pafupi - fupi kwa caka cathunthu , ndipo izi zinatipatsa mwayi wowonjezela zocita pa nchito yathu yolalikila . Ngati mungayende naye pamodzi , ndiye kuti dzanja lake lamanja lingagwile dzanja lanu lamanzele . Ganizilani za maselo . Maselo onse amoyo ni opangiwa mwapamwamba kwambili kuposa nyumba iliyonse , cifukwa amatha kudziculukitsa . Misonkhano ikuluikulu inatithandiza kukonzekela cisautso cimene cinali kubwela N’naganizila za mmene mkazi wanga angadzamvelele pondiona nikuceza mokopana na mkazi wina . Ngati mutapa msangamsanga , simungatape madzi ambili amene mufuna . Iwo amafuna kungomudzidzimutsa munthu na mphatso yoyenela . Conco , Luka ayenela kuti anathandiza mpingo watsopanowo . Ndipo kuti awathandizile kuona kufunika kwa nchito imeneyi , iye anati : “ Ndithudi ndikukuuzani , wokhulupilila ine , nayenso adzacita nchito zimene ine ndimacita , ndipo adzacita nchito zazikulu kuposa zimenezi , cifukwa ine ndikupita kwa Atate . ” ( Yoh . Kodi Yehova anacita bwanji zimenezi ? 13 : 1 , 2 ; Hab . ( Aefeso 1 : 18 ) Izi zimatilimbikitsa kuyamba kutengela zitsanzo za anthu okhulupilika akale ndi a masiku ano , amene anaonapo mmene Yehova anathandizila anthu ake . Zotulukapo zake zinali zakuti Hans anayamba kuŵelenga zofalitsa zathu , anaphunzila Baibo , mpaka anabatizika . Pokambilana , tidzaona ( 1 ) mavuto amene anakumana nawo ndi ( 2 ) mmene tingatengele cikhulupililo cawo ndi kumvela kwawo . Tingacite bwino kusintha ndandanda yathu kuti tizifikila anthu panthawi yoyenela . Pamene Hana anali kupeleka Samueli ku cihema kuti azitumikila Mulungu , anapemphela kuti : “ Yehova . . . ndi Wotsitsila Kumanda , ndiponso Woukitsa . ” ( 1 Sam . Koma Davide sanali kuganiza mwanjila imeneyi . Dzifufuzeni kuti mudziŵe mmene umunthu wanu ulili tsopano komanso mtundu wa munthu amene mufuna kukhala , mwa kuona zimene mumacita bwino , zimene simucita bwino , komanso zimene m’makhulupilila . Koma kwa munthu woyamikila , mphatsoyo ingakhale yamtengo wapatali , komanso yothandiza kwambili . Njila imodzi imene tingaonetsele kuti ndise acifundo ni mwa kukhala wokonzeka kukhululukila ena . Kodi tingacite ciani kuti tithetse mavuto obwela cifukwa cokhala kutali ndi banja lathu ? Mumaŵelenga kalata yonse osati mbali yocepa cabe . Hachi yofiila ngati moto , imene wokwelapo wake ali ndi mphamvu ‘ yocotsa mtendele padziko lapansi . ’ ( Mateyu 11 : 28 - 30 ) Cifukwa cakuti anali waubwenzi ndi wokoma mtima kwa onse , anakwanilitsa lonjezo lake lotsitsimula anthu ofunitsitsa kuphunzila kwa iye . Tikakhala oleza mtima , timaonetsa kuti timakonda anthu ena . “ Musaganize kuti ndinabweletsa mtendele padziko lapansi , sindinabweletse mtendele koma lupanga . ” — MAT . Ndi mwai waukulu kuuza anthu coonadi ca Baibulo ndi kuwaona akucimvetsetsa . Mawebusaiti na mapulogilamu amenewa ni osaipitsidwa na dziko la Satana , ndipo sipakhala zotsatsa malonda . 32 Kodi Mukukumbukila ? “ Acipani ca Herode ” anayambitsa nkhaniyi poganiza kuti ngati Yesu angakambe kuti Ayuda asamapeleke msonkhowo , Aroma adzamuimba mlandu woukila boma . ( Aroma 12 : 9 ; 2 Akor . 6 : 6 ) Izi zitanthauza kuti cikondi ceni - ceni cimakhala cocokela pansi pamtima , osati conamizila cabe . KULALIKILA uthenga wabwino wa Ufumu inali nchito yofunika kwambili kwa Yesu . ( Ŵelengani Salimo 142 : 2 . ) Kodi Yehova anaonetsa bwanji kuti anali kuona zimene Mariya anali kucita ? Baraki ndi gulu lake sanavutike ndi mvula imeneyi cifukwa anadziŵa kumene inali kucokela . M’bale wina amene watumikila monga wothandizila kwa zaka 20 nayenso anati : “ Umenewu ndi mwai waukulu koposa umene sindinauyembekezele . ” M’bale amene anakhumudwa uja anafotokoza zimene zinacitika pakati pa iye ndi woyang’anila wakale . Mau ouzilidwa a mu Salimo 37 aonetselatu kuti anthu amene ‘ ayembekezela Yehova , ndi kusunga njila zake ’ ali na tsogolo labwino . Monga mmene taonela m’nkhani zapita , Mau a Mulungu angatithandize kulimbana na mavuto amene tonsefe timakumana nawo tsiku na tsiku m’dziko loipali . ( Mac . 4 : 34 , 35 ) Akhristu ena anali kuika ndalama pa mbali kuti nthawi zonse azicita copeleka pocilikiza nchito ya Mulungu . Mfundo ya m’Baibo imene ingatithandize ipezeka pa 1 Akorinto 15 : 33 . 103 : 13 , 14 nimazikonda ngako ! 2 : 24 , 25 . N’zoona kuti ndife opanda ungwilo ndipo timalakwitsa . Kodi dipo imagwilizana bwanji ndi Ufumu wa Mulungu ? Ngakhale zinali conco , n’nakhalabe na mtendele wa m’maganizo . Kumbukilani Mose . Izi zinathandiza anthu ambili amene anali osauka kuti akwanitse kugula Baibo . Anthu wamba anakondwela ngako ataona Baibo yomasulidwa m’cinenelo cawo . Inde , pamaziko a nsembe ya Yesu , Yehova angalandilenso anthu m’banja lake popanda kuphwanya mfundo zake zolungama . Pa nthawi ina , Yesu anauza atumwi ake mau oonetsa kugwilizana pakati pa kumvela na cikondi . Iye anati : “ Amene ali ndi malamulo anga ndipo amawasunga , ameneyo ndiye amene amandikonda . ” ( Yoh . Cotelo , Aiguputo anagwilitsa ana a Isiraeli nchito yaukapolo mwankhanza . Mofananamo , ngati simuleza mtima pofunsa mwana wanu wacinyamata kapena mukum’kakamiza kuti akambe , simungadziŵe bwinobwino zimene akuganiza ndi mmene akumvelela . 1 : 10 , 11 ) M’kupita kwa nthawi , Hana anakhala na pakati , ndipo anabala mwana wamwamuna dzina lake Samueli . Cinthu cacikulu cimene Yesu anaphunzitsa n’cakuti ophunzila ake ayenela kuonetsa cikondi . ( Yoh . Kodi Akristu oyambilila anapindula bwanji panthawi ya mtendele ? 18 : 6 , 21 - 25 ) Kuwonjezela apo , atsogoleli acibabulo ndi aciiguputo sanali kutsatila malamulo a zaukhondo ogwilizana ndi sayansi amene Mulungu anapatsa Aisiraeli . ( Num . Ndiyeno , anauza Rute kuti apitilize kukunkha m’munda mwake . Kodi iye analekadi khalidwe lake lankhanza ? Cimodzimodzinso masiku ano , anthu ambili amaona kuti ciyembekezo cimene timalengeza n’copanda pake . — Mac . Ndinali kumeta ndevu ndi kusambila m’zimbudzi za pa malo ogulitsila mafuta a galimoto . ▪ Khalanibe Okhulupilika ku Ufumu wa Mulungu Komabe , panali ena amene anali kufunika kulimbitsa ubwenzi wao ndi Yehova . Kugwilitsila nchito magazi pa Tsiku Lophimba Macimo , ndiponso lamulo lakuti azithila pansi magazi , n’zogwilizana ndi lamulo limene Yehova anapeleka poyamba kwa Nowa ndi mbadwa zake ponena za magazi . Akristu amacita zimenezi cifukwa cokonda anzao . Tikayamba kuganizila zaciwelewele , tiyenela kucotsa maganizo oipawo mwamsanga . Kodi ulamulilo wake ni waukulu bwanji ? Nili na Maxine ku Puerto Rico titangoloŵa m’banja ndiponso mu 2003 pamene tinakwanitsa zaka 50 m’cikwati Ngakhale kuti Adamu anali wangwilo , anacimwila Yehova ndipo anasiyila ana ake mavuto na citsanzo coipa ca kupanduka . N’nali kukwela tumamotoka na mabasi . Pa nthawi ya nkhondo ya pa dziko lonse imeneyo , Ophunzila Baibulo sanamvetsetse mfundo yakuti Akhiristu sayenela kutengako mbali m’nkhondo . Abalewo ataona zimenezi , modzicepetsa analola kuti Paulo apite ku Yerusalemu . — Mac . Kodi iye anali ndani ? Kuyambila ndili mwana , ndimakonda kuŵelenga , ndipo ndimacita cidwi kwambili ndi cinenelo . Tiphunzilapo ciani pa citsanzo ca Baruki ? Iye anapemphela kwa Atate wake wakumwamba kuti am’thandize kupitiliza kukhala wokhulupilika . Hiroo anakwatila Svetlana mu 2005 ndipo onse akutumikila monga apainiya . YESU anali kucikonda Cilamulo ca Mose . * Anthu onse amene ali pabanja afunika kukhala ololela . Komabe , ana ambili amakhala kutali ndi makolo ao . 4 : 16 ) Yehova angatithandize kudziŵa mmene tingayankhile “ wina aliyense . ” Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo — Mbali 2 Kodi mfundo imeneyi n’nayamba kale kuiseŵenzetsa pa mbali ziti m’moyo wanga ? Zinthu zopanda nzelu zimene Hezekiya anacita panthawiyo zinavumbula “ zonse zimene zinali mumtima mwake . ” ( 1 Akor . 10 : 13 ) Ngati tili ndi nkhawa ndipo tikucondelela Yehova , tingakhale ndi “ mtendele wa Mulungu . ” ( Afil . Ndipo pangano la wansembe monga Melekizedeki , litsimikizila kuti mbeuyo idzatumikila monga wansembe . Ngakhale anthu amene sakhulupilila kuti kuli Mulungu , naonso amaona kufunika kopemphela . Iye atamwalila , Papa John Paul waciŵili , anamulemekeza mwa kumudzodza kukhala woyela mtima . Koma popeza zinthu zacitika kale , palibe cimene ungacite . ” M’fanizo la nkhosa ndi mbuzi , Yesu sanachule mwacindunji za nchito yolalikila . Mwacitsanzo , timalandila malangizo acikondi oticenjeza kuti tisamagwilizane ndi anthu oipa pa Intaneti . Poona kuculuka kwa anthu amene anabwela , opeleka cakudya mu hotela ina onse anasiya nchito nthawi imodzi . Koma n’zosakayikitsa kuti Mulungu ndiye anacititsa kuti kugwe cimvula camphamvu , cimene cinapangitsa magaleta ankhondo 900 kukokoloka . Zinthu zina zimene mungaphunzile pa phunziloli ndi zokhudza “ uthenga wabwino wa ufumu wa Mulungu , ” ndi mmene udzathetsela ziphuphu za m’boma . Kodi mungakhomeleze bwanji Mau a Mulungu mwa ana anu ? Conco , kuti ayale maziko olimba a cidziŵitso ca Malemba , anafunikila kuphunzila mfundo zoyambilila za coonadi ca m’Baibo , kumvetsa bwino tanthauzo la kukhala mtumiki wa Mulungu , ndi kukhala wokonzeka kutsatila ziphunzitso za Yesu . Koma akaona kuti ena sakuwalemekeza , ambili amayamba kucita zinthu zosokoneza mtendele . Izi n’zimene anthu ambili osalambila Yehova amacita . Anabatizika mu 1931 , ndipo anakhala akopotala . * ( Chivumbulutso 11 : 15 ) Ufumuwu sulandila misonkho kucokela kwa nzika zake kuti lipeze ndalama zoyendetsela boma lake . ‘ Iyenso amatiyandikila . ’ — Yakobo 4 : 8 . ( Gen . 17 : 1 , 2 , 19 ) Ndiyeno , Mulungu anauza Abulahamu kuti : “ Ili ndi pangano limene anthu inu muyenela kulisunga , la pakati pa ine ndi inu , ngakhalenso mbeu yobwela pambuyo pa inu . Koma mukunenadi zoona , cifukwa ndi zimene lembali lanena . ( Ŵelengani Akolose 4 : 6 . ) Mwacitsanzo , anthu ali ndi luso lophunzila cinenelo . Mzimu woyela unalimbitsa Yesu . Mkhristu safunika kuba mwanjila ina iliyonse ( Onani palagilafu 5 - 7 ) Koma kodi timakonda Yonatani cabe cifukwa cakuti anali wokhulupilika kwa Davide ? 7 : 1 - 3 ) Iye anaikidwa mwacindunji ndi Yehova kuti acite nchito yaunsembe . ( Ŵelengani Aefeso 4 : 8 , 11 , 12 ) Conco , pamene mkulu wakuyendelani , muziona kuti ni mwayi wophunzilapo kanthu pa nzelu zake na malangizo ake . Koma kodi Yehova akatifufuza , amaona kuti tikum’tumikila ndi mtima wathunthu ? N’cifukwa ciani sitifunika kubwelela m’mbuyo pamene takumana na mavuto ? Modabwa , munthuyo anauza Peter kuti , pano wafika ni panyumba ya arabi aciyuda . Komabe , panali zovuta zina . ( Luka 7 : 11 - 15 ; Yoh . 11 : 38 - 44 ) Cifundo cimene Yesu anaonetsa Lazaro mwa njila imeneyi , ciyenela kuti cinacititsa Lazaro kuti akhale ndi mwai wodzalandila moyo kumwamba . Mngelo Gabirieli anauza Mariyayo kuti Mulungu ‘ anamukomela mtima . ’ Izi ziphatikizapo kutaila nthawi yathu yambili pa zinthu za m’dzikoli . Komanso , timakhulupilila kuti Yehova ni wokonzeka kuyankha mapemphelo athu tikamupempha kuti atithandize kupilila mavuto aliwonse amene tingakumane nawo polalikila uthenga wabwino wa Ufumu . ( Afil . Kodi kucita phunzilo laumwini n’kofunika bwanji ? Pasanapite nthawi yaitali , Ayuda akuukila Aroma ndi kupha asilikali aciroma mu Yerusalemu ndipo ayamba kudzilamulila . N’kutheka kuti abale ndi alongo ena panthawi ina anali monga anthu a ku Korinto . Popeza kuti a 144,000 anali anthu opanda ungwilo , io adzamvetsetsa anthu amene io adzalamulila . Ndiponso , kaya tiyesetse bwanji , tsiku lililonse tifunikila kupempha cikhululukilo cifukwa ca cidetso ciliconse . Ndipo tiyenela kuzindikila kuti ndife ocimwa , ndi kuti kudziŵika ndi dzina loyela la Mulungu ndi mwai waukulu . — Ŵelengani 1 Yohane 1 : 8 , 9 . Apa Baibo imaonetsa bwino kuti anthu sanalengedwe ndi mzimu umene sukufa iyai . Adamu anali kukondwela kwambili kuyang’ana mitengo yocititsa cidwi , tumadzi tukutsetseleka m’tumitsinje , ndi nyama zikuseŵela . Malemba a Ciheberi amaonetsa kuti ndiye yekha amene anatumikila monga mfumu komanso wansembe . Koma malinga ndi zimene tapitamo , taona kuti cinthu cofunika kwambili tikakhala ndi nkhawa , ndi kukhulupilila Mulungu . Kenako , pambuyo pokoka mpweya kamodzi kokha , kambani mau a m’kaciganizo kamodzi na mphamvu ya mau yofananayo . Conco , tonse tifunika kukumbukila cenjezo lakuti : “ Amene akuyesa kuti ali cilili asamale kuti asagwe . ” — 1 Akor . ( 1 Yoh . 2 : 12 ) Komanso , kaamba ka cifundo cake , tili na ciyembekezo codalilika cakuti posacedwa tidzaloŵa m’dziko latsopano . “ Cifukwa ca [ Mulungu ] tili ndi moyo , timayenda ndipo tilipo . ” Gail amacita zinthu mogwilizana ndi zimene amakhulupilila mwa kugwila nchito yodzipeleka monga mlaliki wa nthawi zonse . Iye amauzako anzake za lonjezo la Mulungu limene lidzakwanilitsidwa mtsogolo lakuti “ imfa sidzakhalaponso . ” Kodi akaidi aŵili a ku Iguputo amene anafotokozela Yosefe maloto ovuta , zinthu zinawayendela bwanji ? Ma IUD okhala na kopa : Monga takambila kale , cioneka kuti tuzipangizo twa IUD tumalepheletsa mbeu ya mwamuna kukwela m’cibalilo kukafika kumene kuli dzila la mkazi . Hananiya , Misayeli , Azariya ndi Danieli , anatengedwa ku ukapolo mu 617 B.C.E . ( Ezara 5 : 6 , 7 , 11 - 13 ; 6 : 1 - 3 ) Conco , Tatenai analamulidwa kuti asawasokoneze , ndipo anamvela . — Ezara 6 : 6 , 7 , 13 . Cilamulo cinali kukumbutsa Aisiraeli kuti ndi opanda ungwilo . Pamene Yosefe anali ndi zaka 17 , umoyo wake unasintha kwambili . Kodi aliyense wozindikila angakhale waphindu kwa iye ? Zambili zimene tinaphunzila pa misonkhano ija sinizikumbukila , kupatulapo moni wanu . Munthu sangakwanitse kuvula umunthu wakale mwa mphamvu zake cabe . Ganizilaninso za banja lina ku Japan . Ndili wacinyamata , ndinayamba kukonda masewela a zibakela . Kodi inu mumatengako mbali pa nchitoyi ? Zosangulutsa zambili zimacititsa anthu kuona zinthu zoipa zimenezi monga zabwino ndi kusukulutsa mfundo za Yehova za makhalidwe abwino . ( Yes . Musakhulupilile zimenezo . Ngakhale kuti amanena kuti bungwe lao limabweletsa mgwilizano ndi kulemekezana , io kweni - kweni samagwilizana pa mfundo imodzi kuti alimbitse cikhulupililo cao . Ifenso tiyenela kupitilizabe kukhala ngati “ cinthu cimodzi cogwilizana ” masiku ano ndiponso m’masiku ovuta amene akubwela mtsogolo . 1 : 5 - 7 , 12 - 16 ; 2 : 1 - 10 . Apa n’zoonekelatu kuti Yehova akutsogolela nchito yolalikila . Funso lotsilizali n’lothandiza ngako . Mavuto amenewa aonetsa kuti dzikoli lili kumapeto ake . M’mipingo ina , anthu anali kulila pa mwambowu , ndipo mwambowu ukatha , onse anali kucoka popanda kunena ciliconse . Atate anasamukila ku Australia kucoka ku Germany mu 1949 . 24 : 12 . Ndimaona kuti ndinali ndi mwai waukulu kuphunzitsidwa ndi m’bale wodzozedwa amene anali kudziŵana ndi M’bale Charles T . Ku nchito kwawo , anthu sanali kumukonda ngati mmene anali kukondela anzake a ku Japan komweko . Pamene zinthu zikuipila - ipila masiku ano otsiliza , tonse tifunika kukhalabe maso . Koma maka - maka dalilani Yehova . Mofanana ndi zimenezi , tiyenela kuyamikila kwambili Yehova ndi Yesu cifukwa ca dipo . Cifukwa ca ciwembu ca abale ŵake , ndiponso pambuyo pake kunamizilidwa ndi mkazi wa mbuye wake , Yosefe anapezeka kuti ali m’ndende ku Iguputo . Kucita kulambila kwa pa banja ndi phunzilo laumwini nthawi zonse kudzakuthandizani kutsatila miyezo ya Yehova pa umoyo wanu ndi kuthandiza ena . Cilamulo cinatha nchito pamene pangano latsopano linayamba kugwila nchito . ( Aheb . Anthu ena angakambe kuti : “ Munthu safunikila kutsogoleledwa na gulu . 6 : 6 , 7 ) Mwina ena anaphunzila coonadi cifukwa cakuti mtumiki wina wa Yehova anawalalikila . — Aroma 10 : 13 - 15 ; 1 Tim . Mkristu mnzathu angatiuze kuti timwe mankhwala ena ake a kucipatala kapena azitsamba . Amafunanso kuti timudziŵe ndi kum’khulupilila . — Ŵelengani Salimo 19 : 7 - 11 ; Miyambo 1 : 33 . Nthawi zina , mauwo anali kusiyana pang’ono ndi mau a Ciheberi coyambilila . Timadziŵa kuti iye amatiyang’anila ndipo amafuna kutithandiza . NYIMBO : 17 , 13 Caka ciliconse nikatsekela sukulu , n’nali kukonda kucitako upainiya wapachuthi ( tsopano timati upainiya wothandiza ) . Zosangalatsa zambili masiku ano zimalimbikitsa makhalidwe oipa ngati amene anali mu Sodomu na Gomora . Kodi Ahabu anacita ciani atamva uthenga waciweluzo wocokela kwa Yehova ? Pamene udzatuluka , udzakhala utakalamba ndiponso udzakhala wekha - wekha . ” Iye anayamba kukhala bize kugwila nchito yofunika yodzipeleka . Ndipo tingakhale otsimikiza kuti Atate wathu wacikondi amayamikila kuyesayesa kwathu kuti timumvele . Timakhala ndi mwai woonetsa kuti timakonda abale ndi alongo athu . Sin’nali kufuna kuti ubwenzi wathu uthe . “ Ndinapemphela kwa Yehova mosalekeza kuti andithandize kusankha zinthu mwanzelu . ” — Kwabena wa ku Ghana N’nali Kukhulupilila Kuti Kulibe Mulungu ( A . N’nawauza kuti “ Inde , nidzabwela . ” Anthu onse amene amapezeka pa misonkhanoyi amakhala kuti aitanidwa ndi Yehova ndi Mwana wake . Koma naonso angacondelele Yehova kuti apitilizebe kuwathandiza ndi kuwasamalila . Odzozedwa amene ni okhulupilika sadzafunikila cizindikilo cimeneci kuti apulumuke . Ndinali kudzifunsa kuti : ‘ Yehova ndani ? Iwo anali atamvelapo kuti Yerusalemu unali mzinda wokongola kwambili poyamba . Kumeneko , tinayamba kuceza na banja lake uku tikumwa khofi . Patapita nthawi , Baraki anafika kwa Yaeli kukafunafuna mdani wake ameneyu . Tsimikizani mtima kumamatila ku gulu la Yehova ndi kucilikiza mokhulupilika anthu amene waika kuti azititsogolela , ngakhale kuti angalakwitse zinthu zina . N’cifukwa ciani akulu afunika kuphunzitsa ena mumpingo ? Pa cifukwa cimeneci , Yehova analamula kuti mizinda ya Sodomu na Gomora iwonongedwe . Anthu aubwenzi umatha kulankhula nao . Anthu a ku tauni anali kukaseka cifukwa coganiza kuti kanali mbuli . Ngati umu ni mmene inunso mumamvelela , dziŵani kuti pamene Yehova anakukhululukilani , anaiŵalako za chimo lanu . Kodi nanunso angakutonthozeni ? Nthawi zina , ofufuza golide amapeza golide wambili , umene angaugulitse madola ambili . Nowa anakhulupilila zimenezi , ndipo anamanga cingalawa . ▪ “ Anthu Amene Mulungu Wao Ndi Yehova ” Muziyesetsa kuona mmene uphunguwo ungakupindulitsileni m’malo moganizila zolakwika mu uphunguwo , kapena zofooka za woupeleka . Mothandizidwa ndi Mau a Mulungu ndi mzimu wake woyela , Ribeiro anakwanitsa kuvula umunthu wake wakale . Iye anabatizika , ndipo pano tikamba ni mkulu mumpingo . Pa nkhani za anthu amenewa , tidzaphunzilapo mfundo zofunika zimene zingatithandize kukhalabe okhulupilika kwa Yehova pa ciliconse . 1 : 18 ; 1 Pet . Tiyeni tipitilizebe kukhala atumiki ake okhulupilika ndi kulengeza za Mfumu ndi Ufumu wake . Cifukwa cakuti iye monga Mesiya , anali atayamba kale kusonkhanitsa ophunzila amene anali kudzamvela lamulo lotsatilali : “ Mulungu ndiye Mzimu , ndipo onse omulambila ayenela kumulambila motsogoleledwa ndi mzimu ndi coonadi . ” N’cifukwa ciani ndife otsimikiza mtima kuti Yehova amakonda anthu ake ? Anthu ena amene amacita chimo , angakhale akumvabe kuti ali pa ubwenzi wolimba na Yehova . Citsanzo caciŵili ndi cokhudza mmene timagaŵila magazini athu . ( Aheberi 6 : 12 ) Tiyeni titsanzile Yefita ndi mwana wake mwa kukhalabe okhulupilika . Tikatelo , Yehova adzatidalitsa . N’cifukwa ciani Aisiraeli anaona kuti analibe kothaŵila ? ( b ) Ngati Mkhiristu alingalila zosudzula mnzake , kodi afunika kuganizila mfundo ziti ? Anthu ocokela mu fuko lililonse , cinenelo ciliconse , mtundu uliwonse , ndi dziko lililonse . ( Luka 1 : 30 - 33 ) Yehova anapeleka malangizo acindunji onena za mzele wobadwila Mesiya . Iye anakamba kuti mbeu imeneyi ya Davide idzakhala ‘ yoyenelela mwalamulo ’ kukhala Mfumu ya Ufumu wa Mesiya . ( Ezek . Kuti titsanzile cikondi ca Mulungu , kodi tiyenela kucita zinthu motani ndi anzathu ? Kodi zimenezi zinatanthauza kuti Yehova sadzakwanilitsa lonjezo lake ndi kuti walephela kulamulila anthu padziko lapansi ? “ Munthu angathe kucita zinthu zambili pa umoyo wake . 29 Kodi Tiphunzilapo Ciani pa Zimene Jowana Anacita ? ( b ) N’cifukwa ciani tikukambilananso ziphunzitso zimenezi ? Ngati sitingasamale , tingadzipatule kwa Yehova ndi anthu ake . Ngati muli ndi nthawi , ndingakuonetseni imodzi mwa nkhani zimenezi . Mwacitsanzo , m’munda wa Edeni , Yehova anapeleka malangizo omveka bwino otsogolela anthu ku moyo wosatha ndi wacimwemwe . Mu ulosi wake wonena za masiku otsiliza , Yesu anakamba kuti anthu “ adzakomoka cifukwa ca mantha ndi kuyembekezela zimene zicitikile dziko lapansi kumene kuli anthu , pakuti mphamvu zakumwamba zidzagwedezeka . Wacicepele amene wabatizika , amakhala kuti anadzipeleka kwa Yehova . Tisaiŵale kuti cakudya conse cakuuzimu cimacokela kwa Yehova . 3 , 4 . ( a ) Ndi lamulo lotani limene Mulungu anapeleka kwa Adamu ndi Hava ? Abale ena akuthandiza panchito yoonjezela nyumba zina za Beteli ku Wallkill . Ndipo enanso ambili adzipeleka kukathandiza panchito yomanga likulu lathu ku Warwick . Iye anafotokoza kuti : “ Zimenezo zinakhudza kwambili ana athu cakuti anali kumasuka kukamba nafe akakhala ndi vuto . ” Anakambanso kuti : “ Njila yabwino yophunzitsila ena ndi kugwila nao nchito mu ulaliki . Nanga bwanji imwe ? Ni zinthu ziti zimene Wamphamvuyonse wakucitilani zoonetsa kuti “ nzelu zake zilibe malile ” ? Iye ataona kuti a Mboni za Yehova ayankha mafunso ake mwa kuseŵenzetsa Baibo , anazindikila kuti wapeza coonadi . ( Gen . 4 : 8 ) Ndiyeno mbadwa zina za Adamu zinakalamba ndi kufa . Josephus wolemba mbili ya Ayuda , anafotokoza kuti asilikali aciroma analanda nsanja ya Antonia mu Yerusalemu m’caka ca 70 C.E . , ndi kuukila mzinda wonse . ( Gen . 3 : 12 ) Adamu sanavomeleze kucimwa kwake . Sitidziŵa bwinobwino mmene Satana anaonetsela Yesu kacisi . Iwo acita zimenezi ngakhale kuti dzina la Mulungu limapezeka nthawi zokwanila 7,000 m’mipukutu yoyambilila ya Baibulo . Aliyense wa ife afunika kupanga cosankha cacikulu . Omvela a Yesu ambili sanamvetsetse pamene iye anagwilitsila nchito mau ophiphilitsa akuti “ mkate ” ndi “ mnofu . ” Iye anaona kuti zimene Aisiraeli anacita kunali kum’pandukila komanso kutsutsa ulamulilo wake , osati kutsutsa Mose cabe . Akulu amenewa ndi ena amatsatila citsanzo ca Onesiforo . Iye anali kusamalila banja lake , koma anapelekanso thandizo lofunikila kwa Paulo . — 2 Tim . Pambuyo pake , Sauli analola mtima wodzikonda ndi kunyadakuyamba mwa iye monga dzimbili . Pambuyo pake , Petulo anakamba momveka bwino kuti : “ Ameneyu ndiye ‘ mwala umene inu omanga nyumba munauona ngati wopanda pake , umene tsopano wakhala mwala wofunika kwambili wapakona . ’ ” — Mac . 3 : 15 ; 4 : 5 - 11 ; 1 Pet . Yehova anapeleka Cilamulo ca Mose kwa Aisiraeli kuti awaphunzitse mmene anayenela kukhalila ndi mmene anayenela kum’lambilila . Conco , sumikani maganizo anu pa zimene Yehova walonjeza , ndipo musalole ciliconse kukumanitsani mphoto ! 1 : 5 - 8 ) Njila imodzi imene mungacitile zimenezo ndiyo kulambila kwa pabanja kokhazikika . Mwacitsanzo , yelekezelani kuti anthu ena apandukila boma limene limazunza kwambili anthu , kuphatikizapo Mboni za Yehova . ( Yohane 13 : 34 , 35 ) Izi zinali zosiyana kwambili na mmene zinalili kuchechi kwathu . 6 : 14 , 15 ) Tingaonetsenso kuti takhululuka na mtima wonse mwa kupemphelela anthu amene atilakwila . — Luka 6 : 27 , 28 . Ngakhale kuti tili ndi zifukwa zokhalila osangalala , atumiki ena okhulupilika a Mulungu amavutika ndi maganizo olakwika . ( Rute 2 : 2 - 18 ) Mulungu anadalitsa Rute m’njila inanso kuonjezela pa zinthu za kuthupi zimene anam’patsa . Sitifunikanso ‘ kukonda dziko [ la Satana ] kapena zinthu za m’dziko . ’ ( 1 Pet . 5 : 6 ) Njila imodzi yofunika imene mkazi wogonjela amaonetsela kuti amalemekeza ulamulilo wa Yehova ndi kukhala wogwilizana ndi mwamuna wake ndiponso wothandiza m’banja . ( a ) Pelekani zitsanzo za m’Baibulo zimene zingalimbikitse wophunzila kuti akule mwakuuzimu . ( b ) Kodi akulu amakhala ndi colinga cotani akamaphunzitsa ena ? ( 2 Sam . Mwacitsanzo , makolo ena amaopa kulimbikitsa ana awo kucita upainiya , kukatumikila kosoŵa , kukatumikila pa Beteli , kapena kugwilako nchito yomanga nyumba zolambilila . Acinyamata amene amakonda Yehova ndi kumvetsetsa tanthauzo la kudzipeleka , sanyalanyaza kupeleka moyo wao kwa Mulungu ndi kubatizidwa . Panthawiyo , Yosefe , akali na cisoni cacikulu anabwelela mwamsanga ku malo amene Yesu anaphedwela . — Maliko 15 : 42 - 45 . Baibulo limakamba kuti : “ Tiyeni ticitile onse zabwino , koma makamaka abale ndi alongo athu m’cikhulupililo . ” Ndithudi ! ( Mlal . 7 : 16 ) Fanizo limeneli limatiphunzitsanso phunzilo lina . Yoyamba , Yehova nthawi zonse amadziŵa anthu amene amam’tumikila mokhulupilika . Ndipo munawasandutsa mafumu ndi ansembe a Mulungu wathu , moti adzakhala mafumu olamulila dziko lapansi . ” — Chivumbulutso 5 : 9 , 10 . Pambuyo pake , amalume a Nick , anayamba kutisunga , ine na azibale anga . ( Yak . 5 : 11 ) Pa zaka zonsezi , iye anakhalabe wokhulupilika kwa Yehova . Alona Taona mmene Yehova watitetezela , ndi kutitsogolela mobwelezabweleza mwa njila imene sizikanacitika tikanasankha umoyo wa wofuwofu . Pa misonkhano yathu , timalandila malangizo a mmene tingagwilitsile nchito mwaluso zida zimenezi . Cifanizilo cogoba ca ku asuri ca nduna Ndiyeno , zopelekazo amazipangila bajeti , na kuzigwilitsila nchito mogwilizana na colinga cake . Masomphenya a ulosi amenewa akamba za nthawi imene Ufumu wa Mulungu , wopangidwa na Yesu pamodzi na anthu amene adzaukitsidwila kumwamba , udzacotsapo ulamulilo wa Satana ndi kupanga dziko lapansi kukhala paradaiso . TSAMBA 28 • NYIMBO : 72 , 63 Kodi Akristu acikulile ayenela kusangalala ndi ciani ? Nanga citsanzo ca Paulo cingawalimbikitse bwanji ? Kucita zimenezi kungasokoneze ubwenzi wathu ndi Yehova . Ndipo yesetsani kupita patsogolo kuuzimu mwa kuphunzila Baibulo . Kodi n’ndani amene tifunika kuwaonetsa kwambili mzimu woceleza ? ( Akol . 4 : 6 ) Tiyenela kupempha Yehova kuti atipatse mzimu wake woyela kuti utithandize kukhala ofatsa ndi okoma mtima pokamba na abululu athu . Nthawi imene iye anali kulengeza zimenezo , macenjezo okhudza kuonongedwa kwa mzindawo anali atapelekedwa kwa zaka zambili . Olo kuti panthawiyo n’nali cabe na zaka 13 , inenso n’nali kufuna kuyamba upainiya . ” Conco , pokamba ndi anthu , Mulungu amasintha ndi kugwilitsila nchito cinenelo cimene anthuwo angamve mosavuta . Ndiyeno ganizilani izi : Kukanakhala kuti Mulungu anatilenga kuti tizikhala na moyo kwa zaka zocepa cabe , kodi akanalenga anthu na makhalidwe apadela monga amenewa , amene timafuna kukhala nawo na kuwakulitsa kwamuyaya ? Kenako , anayamba kugwila nchito ya umishonale na Paulo . M’zaka ziŵili zotsatilapo , akulu oposa 12,000 analoŵa m’sukulu imeneyi ku Patterson ndi ku Beteli ya ku Brooklyn . Ngakhale zinali conco covalaco cinali kumuteteza ku lupanga kapena mivi ya adani kuti isavulaze mtima wake kapena ziwalo zina zofunika kwambili za thupi . Ndithudi ! Cimacitila umboni kuti maulosi a m’Baibo ni odalilika , komanso azoona , ndiponso ni ouzilidwa na Mulungu . — 2 Petulo 1 : 19 - 21 . Ŵelengani Mateyu 6 : 31 , 32 . Pokhala anthu opanda ungwilo , tonse timalakwitsa nthawi zina . Ngati mkwiyo wakula mphamvu ndipo munthu alephela kuulamulila , ukhoza kusokoneza mtendele wa mpingo . 6 : 3 - 8 . ( Mateyu 24 : 36 ; 25 : 13 ) N’cifukwa ciani tifunika kukhalabe maso ? Ndinayamba kukhulupilila kwambili Yehova ndi Baibulo ndipo ndinali kukhala wosangalala . 8 : 23 ) Pa Salimo 45 : 12 , “ amuna 10 ” ophiphilitsa amenewa akuchedwa “ mwana wamkazi wa ku Turo ” ndiponso “ olemela pakati pa anthu . ” Conco tinaongolela . Kwa zaka zambili akatswili ena a Baibulo anali kukaikila kuti Pontiyo Pilato anali munthu weniweni . Ulamulilo wake unasokonezedwa pamene mtengo unadulidwa ndi kusiidwa kwa nthawi zokwanila 7 , atacita misala . Tikathandiza munthu kuphunzila mpaka kufika pobatizidwa ndiye kuti tathandiza kukulitsa paladaiso wauzimu . — Yes . Amunawo avala mashawelo a kotoni osoka ndi manja a ku dela limenelo ( Mateyu 7 : 12 ) Mwacitsanzo , si cikondi kutumila ena nkhani zoipa zokhudza anthu ena . ( Mika 4 : 2 , 3 ) Conco Akristu oona mungawadziwe mwa kuona mmene amaonetselana cikondi . — Ŵelengani Yohane 13 : 35 . Kusintha kwa zinthu m’banja kungacititse kuti mukhale ndi maganizo osoŵetsa mtendele monga cisoni ndi kukhumudwa . Padziko lonse lapansi , mamiliyoni a tumapepala twauthenga , tumabuku , ndi magazini zimagaŵilidwa panchito yapadela kwaulele . ( Gen . 3 : 23 , 24 ) Panthawi imodzi - modziyo , Mulungu anaonetsa cikondi cake monga tate mwa kutsimikizila kuti cifunilo cake cidzakwanilitsika . N’cifukwa ciani tifunika kukhala ogwilizana ? Zambili n’zogamphuka - gamphuka , zophwanyika , komanso zosaoneka bwino . Pa usiku wakuti maŵa aphedwa monga cigaŵenga , Yesu moona mtima anauza ophunzila ake kuti anali “ kumva cisoni cofa naco ” cifukwa ca mavuto amene anali kudzakumana nao . Pamene n’nali kusinkha - sinkha pa zimenezi , n’napezeka m’ngozi ya honda moti anan’cita adimiti ku cipatala . Onse amuna ndi akazi anali ofunitsitsa kuŵelenga mau a Yesu m’cinenelo cawo . ( Yohane 14 : 30 ) Mtumwi Yohane nayenso analemba kuti “ dziko lonse lili m’manja mwa woipayo . ” — 1 Yohane 5 : 19 . Komabe , tifunika kucita khama . Kodi izi n’zoona ? 15 Muziyamikila Kuolowa Manja kwa Yehova Ca m’ma 1980 , mlongo Wendy anapita ku dziko lacisumbu la Vanuatu , pamtunda wa makilomita 1,770 kum’maŵa kwa Australia . Malemba ena amanena kuti ulamulilo wa Yehova , kukoma mtima kwake kosatha , cilungamo cake ndi coonadi cake zidzakhala kosatha . ( Eks . 15 : 18 ; Sal . Pa Pentekosite mu 33 C.E . , Yehova anaonetsa kuti amafuna kuti uthenga wabwino ulalikidwe padziko lonse lapansi . Cinali covuta kuti Didier na Nadine aphunzile citundu ca Cimalagase . Iye anati : “ Ndimagwila nchito mogwilizana ndi thanzi langa , ndipo ndimapuma mobwelezabweleza . Ena anacita khama kumasulila Baibulo m’zinenelo zimene anthu anali kumva mosavuta . Yesu anakamba kuti “ Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha , kuti aliyense wokhulupilila iye asaonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” 6 : 10 . 143 : 5 ) Koma kukumbukila Mlengi wathu Wamkulu kumaphatikizapo kusinkha - sinkha zimene iye amafuna kwa ife . Muziganizila kwambili zimene muŵelenga ndi kuyelekezela kuti mukuona zimene zicitika M’malo mofunsila kwa Yehova kuti awauze zocita , io anati : “ Tiyeni tikatenge likasa la pangano la Yehova ku Silo , kuti likhale pakati pathu ndi kutipulumutsa m’manja mwa adani athu . ” Timadziŵa kuti Mdyelekezi aliko cifukwa cakuti ndiye anakamba ndi Hava kudzela mwa njoka . ( Gen . 6 : 4 ) Kodi nkhani imeneyi ni yaikulu bwanji ? Mashini opulinthila akalibe kufika ku America , anthu anali kucitolemba pamanja makope a Baibo . 37 : 36 , 37 . Ndiye cifukwa cake , Baibo imatikumbutsa kuti : “ Samalani kwambili kuti mmene mukuyendela si monga anthu opanda nzelu , koma ngati anzelu . Muzigwilitsa nchito bwino nthawi yanu cifukwa masikuwa ndi oipa . ” Koma zinanipatsa mwayi wocitila umboni . ( Rute 2 : 13 ) Ngati alendo aonetsa khalidwe labwino limeneli , amalemekezedwa ndi anthu a m’dziko lacilendo , ndi okhulupilila anzawo . Bwanji ngati Habakuku akanakhumudwa ndi kuyamba kuganiza kuti : ‘ Kwa zaka zambili , ndakhala ndikumva kuti Yerusalemu adzaonongedwa . Ndipo adani athu Satana na ziŵanda , ni amphamvu . Paulo atawaona capatali “ anayamika Mulungu , ndipo analimba mtima . ” ( Mac . Cikondi “ cimayembekezela zinthu zonse , ” kuphatikizapo zakuti anthu amene anasiya Yehova adzabwelela kwa iye . Yehova anadalitsa zaka 10 zoyambilila za ulamulilo wa Asa mwa kum’patsa mtendele woculuka . Nanga pangakhale zotulukapo zanji ? Monga mmene Aisiraeli anakhalila na nkhawa cifukwa ca kucedwa kwa Mose pa Phili la Sinai , Akhristu ena masiku ano angakhale na nkhawa cifukwa coona ngati kuti tsiku la Yehova laciweluzo ndi dziko latsopano zacedwa . Kondwelani , dumphani ndi cimwemwe , cifukwa mphoto yanu ndi yaikulu kumwamba , pakuti umu ndi mmenenso anazunzila aneneli amene analipo inu musanakhaleko . ” Komabe , cifukwa ca kupanda ungwilo , mmene tinaleledwela , na zifukwa zina , nthawi zina cimativuta kulandila cilango kapena kuciona moyenela . Nchito imeneyi inayamba mu 1914 , mpaka kuciyambi kwa 1919 . Iwo amazunzidwa kwambili cifukwa comvela malamulo a Mulungu mokhulupilika . Kulimbana ndi nkhawa za paumoyo ( Miy . 30 : 8 , 9 ) Kaya munthu waba pa cifukwa canji , kuba n’kuba ndithu . Munthu wakuba amaona zinthu zakuthupi ndiponso cikhumbo cake cadyela kukhala zofunika ngako kuposa kumvela Mulungu . Pa 1 Akorinto 2 : 16 , Baibo imaonetsa kuti tiyenela kukhala na “ maganizo a Khristu . ” Motelo , timam’konda ndipo timafunitsitsa kumvela malamulo ake . Ngakhale kuti dzikoli lili pafupi kwambili ndi dziko la Nepal , maikowa ndi osiyana kwambili . Komabe , kodi timatengeka ndi zosangulutsa za m’dzikoli ? Ine ndiye amene ndimanena kuti , ‘ Zolingalila zanga zidzacitikadi , ndipo ndidzacita ciliconse cimene ndikufuna . ’ ” Kulikonse kumene tinali kusamukila , tinali kupeza a Mboni za Yehova . Kwa mawiki angapo , iwo anali na mwayi wotumikila pamodzi ndi makolo a m’baleyo , amene anali kugwilanso nchito yomanga ku Warwick . Komanso amaona kuti ni dalitso lalikulu kutumikila pa Beteli pamodzi na mwana wawo wamkazi ndi mwamuna wake . Kodi n’cifukwa ciani iye anapita kumeneko ? Ndiyeno , ndinaphunzila coonadi ponena za Yehova , ndipo ndinayamba kum’konda kwambili . Ataona kuti sin’nagonje ngakhale pambuyo poniwopseza ndi kuninyengelela , ananiweluza kuti nikagwile nchito yakalavula gaga kwa zaka 7 m’ndende ina pafupi na mzinda wa Saransk . Abale ena amene akukalamila maudindo mumpingo , mwamacenjela angapusitse akulu n’colinga cakuti awayamikile kukhala akulu . Tikaona cimwemwe cimene anthu amakhala naco akalandila coonadi , timakhala osangalala ngako . ” ( Ŵelengani 2 Timoteyo 3 : 14 - 17 ) ‘ Munaphunzila ’ kwa makolo anu za Mulungu woona ndi zimene muyenela kucita kuti mumukondweletse . Pa cocitikaco , Mose anacita zinthu mwanzelu mwa kuyang’ana kwa Yehova na kutsatila malangizo ake mosamala . N’zosadabwitsa kuti ise anthu a Yehova ndise ogwilizana . Iye anakamba kuti amai ake a zaka 86 omwe anali ndi mavuto athanzi , nthawi zonse anali kucita ulaliki wa pafoni umenewu moti anali kusangalala kwambili kutsogoza phunzilo mai wina wa zaka 92 . Kuti io adalitsidwedi , ayenela kumasulidwa ku ucimo ndi kuwabweletsa m’banja la Yehova . 2 : 24 ) Timafuna kusangalala ndi kupumula , koma ngati tiika ubwenzi wathu ndi Yehova pa malo oyamba timasangalala kwambili ndi zinthu zimenezi . Ndazindikila kuti pali zinthu zina zimene ndinali kucita poyamba zimene tsopano sindingathe kuzicita . ” Koma coyamba tifunse kuti , n’ndani analemba Baibo paciyambi ? Kuona cisamalilo ca Yehova , kunan’thandiza kukhala na cidalilo cakuti inenso adzanisamalila . Conco , “ poona cikhamu ca anthu , iye anawamvela cisoni , cifukwa anali onyukanyuka ndi otayika ngati nkhosa zopanda m’busa . ” ( Mat . Kukula kumatenga nthawi yaitali cifukwa kumayamba pamene mbeuzo zabyalidwa mpaka nthawi yokolola . Panthawi imodzimodziyo , tiyenela kukhala mogwilizana ndi mapemphelo amenewa mwa kucita nao nchito yofunika kwambili imene ndi “ cizindikilo ” cimene cikukwanilitsidwa . ( Deuteronomo 4 : 7 , 8 ) Aisiraeli akanaonetsa kuti amayamikila Yehova mwa kumvela malamulowo . Mwa ici , Barizilai anapeleka mwana wake Chimamu , kuti akakhale kwa mfumu m’malo mwa iye . — 2 Sam . ( 2 Mbiri 16 : 9 ) Iye amatikonda ndipo amatimvetsetsa . Pomaliza , Antonio anati : “ Ngakhale kuti titumikila ku mipingo yosiyana , timakondana kwambili kuposa kale . ” Panalibe makonzedwe a kusudzulana kapena kukwatila cipali yayi . Guest ) , Feb . “ Kuti makolo anu na anthu ena azikudalilani , zimatenga nthawi komanso zimafuna khama . Pamene n’nabadwa , atate anali kuseŵenza kwa mmodzi wa alimiwo . ( a ) Kodi tiyenela kukhala otsimikiza mtima kucita ciani ? Kodi muyenela kuopa kupanga lonjelo limeneli ? Kacisi wauzimu ndi makonzedwe a Mulungu okhudza kulambila koona . Monga abusa auzimu , akulu mu mpingo angathandize makolo pa nchito yophunzitsa ana awo mwa kukamba ndi anawo za ubwino wokhala na zolinga zauzimu . N’cifukwa ciani Yehova nthawi zina sayankha mapemphelo nthawi yomweyo ? A Daka : Kudzela mwa Yesu . Pakati pa anthu amene anayamba kuphunzila nao Baibulo panthawiyo , panali mayi wina ndi ana ake anai . 10 Kukhululuka Akristu odzozedwa amene akali padziko lapansi amasangalala akaganizila kuti posacedwapa adzagwilizana ndi abale ao ndi Mwamuna wao kumwamba . ( 2 Mbiri 11 : 16 , 17 ) Conco , kumvela kwa Rehobowamu kunapangitsa kuti ufumu wake ulimbe . Kodi iye anaphunzitsa bwanji ena ? Mlongo wina dzina lake Helga , akukumbukila kuti kutatsala pang’ono kuti atsilize sukulu , anzake ambili a m’kalasi anali kukamba za zolinga zao za mtsogolo . Iwo anali ndi nyumba yaoyao ndipo analibe ana . Patapita zaka 21 zokha kucokela pamene Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse inatha , nkhondo yaciŵili ya padziko lonse inayamba , ndipo inapha anthu ambili kuposa amene anafa pa nkhondo yoyamba . N’naika maganizo pa zoimba - imba na kujambula zithunzi ndi manja . ( Mateyu 6 : 31 - 33 ) Timam’khulupilila Yehova ndipo tikudziŵa kuti adzakwanilitsa lonjezoli . Oweluza a kukhoti asanapeleke ciweluzo anali kufunika kutsimikizila kuti mlanduwo ndi woona . — Deuteronomo 13 : 14 ; 17 : 4 . Mwacitsanzo , tingamvetsele pamene m’bale kapena mlongo akuyeseza kukamba nkhani yake . Koma sindinali kum’dziŵa . Conco , tikamvela lamulo limeneli , Yehova amakondwela . ( 1 Akor . 4 : 7 ) Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Ndikuuza aliyense wa inu kumeneko kuti musamadziganizile kuposa mmene muyenela kudziganizila . Mwacitsanzo , kwa zaka zambili n’nali na namba yanga ya “ mwayi ” yochovela njuga ya lottery wiki iliyonse . Cina cofunika kwambili ni kupemphela nthawi zonse mocokela pansi pa mtima , maka - maka tikakumana na mayeselo kapena mavuto ena . ( Genesis 25 : 8 ) Pamene anali ndi zaka 175 , Abulahamu anali kukhala wokhutila akaganizila za umoyo wake . Komanso , yesani kudziyelekezela kuti ndinu munthu amene mukuŵelenga m’nkhaniyo . Kupyolela pa Webusaiti yathu , abale ambili amadziŵa za masoka acilengedwe ndi milandu imene imakhudza anthu Yehova . ( 1 Pet . Nkhani ziŵilizi , zidzafotokoza cifukwa cake panafunikila dipo , zimene dipolo linakwanilitsa , ndi mmene tingaonetsele kuti timayamikila na mtima wonse mphatso imeneyi yoposa zonse yocokela kwa Atate wathu wakumwamba . Louis na mkazi wake Perrine , amene ali na zaka za m’ma 30 , anacoka ku France kupita ku Madagascar . Mu 1958 , panapangiwa makonzedwe akuti ku New York City kucitike msonkhano wa maiko . Yobu 28 : 12 , 15 ionetsa kuti nzelu zocokela kwa Mulungu ni zamtengo wapatali kuposa golide na siliva . Paulo anauza Timoteyo kuti : “ Pitiliza kukhala wodzipeleka poŵelenga pamaso pa anthu , powadandaulila , ndi powaphunzitsa . . . . Nthawi zina , anali kukhala kumeneko kwa moyo wake wonse . Ndani angapindule mwa kuphunzila mosamala Nyimbo ya Solomo ? Nanga cifukwa ciani ? 6 : 33 ; Maliko 14 : 8 ; 2 Akor . 24 : 14 ; 28 : 19 , 20 ) Ena ndi atumiki a nthawi zonse ndipo abale okhwima amatumikila ena mumpingo monga akulu ndi atumiki othandiza . “ Mulungu woona anamvetsela mau a Manowa . ” Koma muyenela kusamala kuti musadziikile zolinga za kuuzimu cabe kuti muchuke . Iwo anacita nane zinthu mokoma mtima kwambili kuposa mmene ndinali kuganizila , ndiponso anali kumvetsela mosamala pamene ndinali kuwauza mavuto anga . Komabe , kukhala ndi nkhawa zopitilila muyeso kungatibweletsele mavuto . Ngakhale ndi conco , wacinyamata mmodzi anakamba kuti si Yesu amene amayankha mapemphelo , koma ndi “ Mulungu . ” Ngati n’conco , anawo ayenela kuona zinthu moyenela , mwina angapemphe thandizo . * Mlongoyu amaona kuti ali ndi udindo woyamikila abale . Ndipo caka ciliconse , ana oposa 3,000,000 amene sanakwanitse zaka 5 amafa ndi njala cifukwa cosoŵa cakudya . 103 : 20 ) Angelo ndi apamwamba kwambili kuposa anthu ndipo ali ndi nzelu ndi mphamvu zoculuka . Tsopano , Daniel ali na cikumbumtima coyela , ndipo posacedwa anaikiwa kukhala mtumiki wothandiza . ( Luka 12 : 32 ; Yohane 10 : 16 ) Popeza pali magulu aŵili , ena angadzifunse kuti : ( 1 ) Kodi a nkhosa zina ayenela kudziŵa maina a odzozedwa onse masiku ano ? Posacedwapa , iye adzathetsa umphawi ndi njala . — Ŵelengani Salimo 72 : 16 . Iwo anali kudwala mwakuuzimu . Koma unjikani cuma canu kumwamba . ” ( Mat . Mmodzi wa anzawo atsopano anali Willie Sneddon , amene anacokela ku Scotland , kumenenso makolo anga anacokela . Mneneli wodzicepetsa ndi wokhulupilika ameneyo anapelekadi uthenga wa Mulungu , ndipo Yehova anam’teteza ku mkwiyo wa Yerobowamu . — 1 Maf . Kodi Mark ndi Claire anacita bwanji zimenezi ? Iwo anaona dzanja la Mulungu . Buku la Chivumbulutso limaonetsa kuti angelo adzagwila nchito mwakhama kuthandiza anthu padziko lonse kuphunzila za Yehova Mulungu na colinga cake pa anthu . Ndise okondwa kuti tinapanga cosankha cobwela kuno kudzatumikila Yehova . ” ( b ) Kodi ndani amene adzasangalala ndi cikwati ca Mwanawankhosa kumwamba ? Conco , kuti tikapulumuke tifunika kukhala odzipeleka kwa Yehova Mulungu , kukhala ndi makhalidwe abwino ndiponso kucita zinthu zimene iye amakondwela nazo . ( Mateyu 5 : 3 ) Tiyeni tipitilize kuŵelenga ndi kucita zimene timaphunzila . Kunena zoona cikondi cimene a Mboni za Yehova anandionetsa ndi cimene ndinali kufunika . Ndinu maso ao . ” Kodi zimenezi zinatheka bwanji ? Caputa 2 ya buku imeneyi ili na ulosi wokamba za maboma kapena kuti maufumu amene adzakhalapo mokonkhana - konkhana , kuyambila na ulamulilo wa Babulo wakale mpaka masiku athu ano . Kuganizila zotsatilapo za makhalidwe oipa kudzatithandiza kuti tisalole zilakolako zoipa kutilepheletsa kumva mau a Yehova . Kumvetsela mwachelu na kudziŵa mfundo zonse zokhudza nkhaniyo kungakhale kothandiza kwambili kuti tipewe kuganizila ena molakwa ndi kupewa kulakwitsa zinthu . Wodala ndi munthu amene amacita zimenezi . ” Ngati pali khalidwe limene limachulidwa kaŵili - kaŵili m’Baibo , ni cikhulupililo . Koma zotsatilapo zake zaonetsalatu kuti anthu ndiponso Satana si olamulila abwino . Limakamba kuti : “ Thaŵani kupembedza mafano , ” ndi kuti “ pewani mafano . ” Ndipo andipha ndithu , koma iweyo akusiya wamoyo . Nthawi zonse tiyenela kuyesetsa kukhala oyela potsatila Woyela Koposa , mwini dzina limene timadziŵika nalo . N’cifukwa ciani Yesu anagwilitsila nchito fanizo la wamalonda woyendayenda ndi la cuma cobisika ? Utagogoda , ndinazindikila kuti Yehova wayankha pemphelo langa . ” Zimenezi zidzakuthandizani mukamakonzekela ulendo wobweleza , waubusa kapena nkhani . Komanso kutumikila m’magawo amenewo kumakhala kosangalatsa . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inuyo muwacitile zomwezo . ” — Luka 6 : 31 . Sadzacita zimenezi mwakulanda anthu mphatso ya ufulu wodzisankhila zocita , kuti akhale monga makina amene amangocita zimene anapangidwila . Cikumbumtima cathu ndi umboni wakuti Yehova amatikonda ndipo amatifunila zabwino . Ndipo pa nkhani yoimba imeneyi , Malemba amalangiza anthu a Yehova kuti nthawi zina ayenela “ kufuula mosangalala . ” — Sal . Ndiye cifukwa cake Akhristu salola kucotsa mimba monga njila ya cilezi . ( Ezek . 18 : 23 ) Pa nthawi imodzi - modzi , pamene tilalikila ku nyumba ndi nyumba komanso pa malo ena aliwonse , timacenjeza anthu ambili kuti Ufumu wa Mulungu udzabwela ndi kuwononga dziko loipali . — Ezek . Janet anati : “ Cimene candithandiza kulimbitsa cikhulupililo canga , ndi kuona mmene Yehova wandithandizila . Inde , alikodi . Pokamba za oukitsidwila kumwamba , Baibo imakamba kuti adzaukitsidwa “ aliyense pamalo pake , ” kapena kuti mwadongosolo . ( 1 Akor . ( b ) Kodi lupanga ndi uta zimaimila ciani ? Umoyo wa Davide unasinthilatu atangodzozedwa . ( 1 Akor . 11 : 25 ) Kupyolela mwa mneneli Yeremiya , Mulungu anakambilatu kuti adzacita pangano latsopano losiyana ndi pangano la Cilamulo limene anacita ndi Aisiraeli . Ndi mwambi wotani umene anthu ena amakonda kukamba ? Abale ambili amene atsatila malangizo amenewa apita patsogolo , ndipo ayenelela maudindo mumpingo . Zimenezi zingathandize amene timaphunzila nao Baibulo kusintha makhalidwe ao . Kudalila Yehova kudzatithandiza kukhala okhutila ndi zimene tili nazo . Timaona mmene Yehova walepheletsela zoyesa - yesa za adani zofuna kuletsa nchito yolalikila . ( Onani palagilafu 18 ) Ngakhale zinali conco , ndinaona kuti Yehova akundigwila dzanja ndipo akundilimbikitsa . Panalibe cifukwa coninyozela na kunikalipila . ” Cimeneco ndi cidziŵitso . Koma Helga anakambilana nkhaniyi ndi anzake ofikapo kuuzimu mumpingo . ( Machitidwe 6 : 1 ) Kodi tingadziŵe bwanji kuti tayamba kukhala ndi mzimu wonyada ? Yehova amakudziŵani bwino kwambili kuposa munthu wina aliyense . Nanga tingakulitse bwanji khalidwe la kudzicepetsa , limene lingatithandize pa mayeselo ? Inde , Yehova amacititsa kuti zinthu zooneka monga zosatheka zitheke . Cifukwa cakuti inu mungapulumuke mapeto amenewa . Monga mmene taonela poyamba paja , makamu a kumwamba mogwilizana adzaimba kuti : “ Tiyeni tisangalale ndipo tikhale ndi cimwemwe codzaza tsaya . Timupatse ulemelelo , cifukwa ukwati wa Mwanawankhosa wafika , ndipo mkazi wake wadzikongoletsa . ” ( Chiv . ( Yes . 43 : 19 ) Macaputala 6 oyambilila a buku la Yesaya , anapeleka cenjezo la masoka amene anali kudzagwela Yerusalemu ndi mizinda yake yozungulila . N’ciani cinawathandiza kudziŵa kuti tsopano ndi okonzeka kubatizidwa ? Ndithudi , Yehova amacilikiza aja amene amakhala ndi umoyo wodzimana cifukwa cofunafuna Ufumu coyamba . — Mat . Cifukwa cakuti tinalengedwa m’cifanizilo cake , timatha kuganiza , kupanga zosankha ndi kukhala paubwenzi wolimba ndi ena . — Gen . M’Baibo muli malangizo othandiza kwambili amene ningaseŵenzetse tsiku lililonse . ” Coyamba , anali na alifabeti yacilendo , ndipo caciŵili mau ake anali na mphatikila kutsogolo ndi kumbuyo . Mphatikila zimenezi zinali kupangitsa kuti zikhale zovuta kuti azindikile liu lake lenileni . Munthu wosaona akhoza kudziŵa mthunzi osati monga malo amene palibe dzuŵa koma monga malo amene pamveka kuzizila akacoka pa dzuŵa . ( b ) Kodi kumvela lamulo limenelo kunali kofunika motani ? ( 1 Akorinto 15 : 33 ) Ndiye cifukwa cake timalimbikitsidwa kuti tidzipezeka pa misonkhano nthawi zonse . Kuŵelenga pakuti : “ Yesu anamuuza kuti : ‘ Ine ndine njila , coonadi ndi moyo . ‘ Nanga n’cifukwa ciani umaikhulupilila ? ’ “ Mulungu ndiye cikondi . ” — 1 YOHANE 4 : 8 , 16 . Bungwe Lolamulila limacita zinthu mokhulupilika ndi mwanzelu pogwilitsila nchito zopeleka . ( Mat . ( Yesaya 44 : 27 – 45 : 2 ) Kodi zimene Mulungu analosela zinakwanilitsidwadi ? 5 : 21 - 29 ) Patapita nthawi , akuluwo anayamikila mwamunayo cifukwa ca kuyesa - yesa kwake . Cinanso , Khristu anapeleka “ mphatso za amuna ” ku mipingo , kutanthauza akulu kuti aziŵeta nkhosa za Mulungu . ( b ) Pa zocita zathu ndi ena , tingaonetse bwanji kuti ndise acifundo monga Mulungu ? Mu August 1997 , tinalandila mwayi wa utumiki umene tinali kuulakalaka kwa nthawi yaitali . Monga Mwana wobadwa yekha wa Mulungu , Yesu wakhala akusonyeza citsanzo ca kudzicepetsa kweni - kweni ndi kugonjela ku ulamulilo wa Atate wake . ( Yes . 50 : 4 , 5 ; Yoh . Ngakhale kuti anabatizika , ena nthawi zina amayesedwabe kuti ayambenso makhalidwe oipawa . Zotsatilapo zake zinali zakuti mkazi wanga anayamba kuvutika maganizo , ndipo ine n’nali kudziwona ngati wacabe - cabe . TONSEFE timafooka nthawi zina . Ngakhale kuti iye anali wokongola kale mocititsa kaso , anam’samalila ndi kum’konzekeletsa kwa caka conse . ( Yakobo 5 : 17 ) Kaya maganizo ake anali otani , Baibulo limanena kuti : “ Eliya anapita pamene panali Elisa n’kumuponyela covala cake cauneneli . ” Ndipo kumene ndikupitako , inu njila yake mukuidziŵa . ” — Yoh . 14 : 2 - 4 . Mulungu ni weni - weni kwa iwo . Lemba la Machitidwe 17 : 30 limatiuza kuti : “ Mulungu analekelela nthawi ya kusadziŵa koteloko . ” 3 : 8 ) Inde , tidzalandila madalitso malinga na nchito imene timagwila , osati zotulukapo za nchitoyo . ▪ Tingathe Kupewa Ciwelewele Mfumu Solomo analonjeza Msulami kuti adzam’pangila ‘ zokongoletsa zoti azivala kumutu . Anthu ena otsutsa amanena kuti akazi aciyuda sanali kukhala ndi ndalama kapena zinthu zina zimene zingadziwabweletsela ndalama . Anthu a mitundu adzakhumudwa kwambili ndi zimenezi , ndipo adzalakalaka kuononga odzozedwa a Yehova ndi a nkhosa zina . Anali wamkali , wokayikila ena , ndi wankhanza . Mzimu woipa ukafika pa Sauli , cinthu cimene cinali kumukhazikako mtima pansi ni nyimbo . Masiku ano , anthu ambili amafunitsitsa kukhala na zinthu zimene zili m’fashoni , kaya ni zovala , mafoni , makompyuta , kapena zinthu zina . Mpainiya wina mu mpingo umenewo anati : “ Timavutika kupeza wogwila naye nchito masana . ” “ Palibe munthu angabwele kwa ine akapanda kukokedwa ndi Atate . ” — YOHANE 6 : 44 . 5 : 19 . Gawo yaconde imeneyi ni yokondwelatsa kwambili kuseŵenzelamo . ” Nthawi zina liu limeneli linali kunena za mwamuna amene ndi wofulidwa . Mwacitsanzo , William ndi mkazi wake Sandra , a zaka za m’ma 60 anali kusangalala ndi umoyo ku Pennsylvania . Mariya , amai ake a Yesu , anapezekapo pa phwandolo . 32 : 34 ) Baibo siikamba kuti Aisiraeli anamuona mwacindunji mngelo akucita zimenezo . Tisakaikile kuti ngati titsatila malangizo a Yehova , iye adzatithandiza . Conco , anthu amene aphunzila mfundo zoyambilila za m’Baibulo , angasankhe zimene afuna . ( Mateyu 24 : 24 ) Akristu odzozedwa sangadziŵe kuti adzalandiladi mphoto yao . Iwo adzadziŵa zimenezi Yehova akadzawaweluza kuti ndi okhulupilika . Ndiye cifukwa cake Yehova ataona anthu akucita cifunilo cake anakamba kuti zonse zimene anapanga “ zinali zabwino kwambili . ” Nanga n’cifukwa ciani kuganizila mmene Yehova wakuthandizilani n’kofunika ? Onse okhulupilika kwa Yehova ndi gulu lake adzalandila madalitso . Mlongo Margaret wa ku England , amene lomba ali m’zaka za m’ma 70 , anatumikila monga mmishonale ku Laos . Iwo anali kupeleka cisamalilo kwa ana a nkhosa osakhwima ndi opanda mphamvu monga mmene nkhosa zazikulu zimakhalila . — Gen . Zimenezo zinakwiitsa kwambili mkulu wa apolisiyo cakuti anamenya pa desiki mwamphamvu mpaka wapolisi wina amene anali m’cipinda cina anathamanga kuti adzaone zimene zinacitika . Kodi kusamba kumene Aroni ndi ana ake anali kucita kunali kuimila ciani ? ( Onani bokosi m’nkhani ino . ) Paladaiso wauzimu amatithandiza kudziŵa bwino anthu amene amalambiladi Mulungu ndi kumutumikila pa kacisi wake wauzimu masiku ano . — Mal . Onani nkhani yakuti , “ Kodi Mungadziwe Bwanji Baibulo Lomasuliridwa Bwino ? ” N’cifukwa Ciani Anthu Amapemphela ? Pamene ndinakhala ndi zaka 12 , ndinathaŵa pa nyumba kwa nthawi yoyamba . Russell atakamba nkhani yapoyela ku Dublin , katswili wina wa zacipembedzo amene O’Connor anam’bweletsa anayamba kufunsa mafunso . Koma M’bale Russell anamuyankha poseŵenzetsa Malemba , ndipo omvetsela anakondwela kwambili . Komanso mfumuyo inadziŵa kuti Mulungu wa Yosefe ndiye anamuthandiza kukamba mau anzelu amenewo . Angelo okhulupilika amakhala kumwamba , ndipo amatha kuona Mulungu mwacindunji . — Luka 24 : 39 ; Mateyu 18 : 10 ; Yohane 4 : 24 . Kodi n’kuti kumene anapeza thandizo ? Yesu anati ‘ tidzadana ndi mmodzi ndi kukonda winayo , ’ kapena ‘ tidzakhulupilika kwa mmodzi ndi kunyoza winayo . ’ Ulosi wa pa lembali umakamba za maulamulilo amphamvu padziko lonse otsatizana - tsatizana mpaka masiku ano . Kodi cosankha cofunika kwambili cimene mungapange paumoyo wanu n’citi ? Kodi mudzacita ciani ngati zotelo zakucitikilani ? Pofunanso kuthandiza aliyense kuti aziimba na mtima wonse , mau ena a m’nyimbozo anasinthiwa kuti akhale osavuta kumva , ndipo ena amene anali kumveka acikale anawacotsamo . Kodi nimayesetsa kucita cifunilo ca Mulungu na mtima wonse ? Ambili mwa anthu amenewa ni acicepele . 3 Tinapeza Nchito Yopindulitsa Kwambili Ifenso timakamba ndi Yehova mwa kupemphela kwa iye kaŵilikaŵili . Iye anati : “ Aliyense wokonda moyo wake akuuwononga , koma wodana ndi moyo wake m’dziko lino akuusungila moyo wosatha . ” ▪ Kodi ‘ Mumakonda Anzanu Mmene Mumadzikondela ’ ? Komabe , pambuyo pakuti Yesu waphedwa na kuukitsidwa , ubatizo unakhala na colinga cina capadela kwa otsatila ake . Tsiku lina masana pa Mande , banja la Ana linakumana ndi vuto lalikulu . Mwacitsanzo , bwanji ngati inu , kapena m’bululu wanu , wadwala matenda aakulu , kapena wakumana ndi zinthu zina zoipa . ( Mat . 23 : 38 ) Yehova anakana Aisiraeli , ndipo m’malo mwake , anasankha mpingo wacikristu kukhala anthu ake . — Mac . 2 : 1 - 4 . ( Chiv . 3 : 19 ) Akulu angacite bwino kutengela citsanzo ca Khristu pamene apeleka uphungu . Mtsikana wina , dzina lake Abigail , amene anabatizika ali na zaka 12 , anati : “ Nimaona kuti Yehova ndiye amene tiyenela kumuyamikila kwambili kuposa munthu wina aliyense m’cilengedwe conse . Jordan anakamba kuti : “ A Russell , bwenzi lacikulile la banja lathu , ni amene ananipatsa pamene n’nali wamng’ono kwambili . ” Kodi tingaonetse bwanji kuti ndifedi “ ophunzitsidwa ndi Yehova ” ? ( 2 Atesalonika 3 : 11 ; 1 Timoteyo 5 : 13 ) Nkhani zina zimakhala zacisinsi . Atate wanzelu amakondwela kusiya motokayo m’manja mwa mwana wake , ndipo safunika kumamulamulilabe . Iwo amazindikilanso mfundo yakuti , kuti apitilize kukhala ndi moyo ndi kusangalala amadalila Mulungu kuti awapatse zinthu zonse zocilikiza moyo monga cakudya , mpweya ndi madzi . Pamene Isaki anali na zaka 5 , banja lonse linakonza phwando lalikulu , kukondwelela kuti mwanayo wasiya kuyamwa . Yehova sangalekelele kuti pakati pa anthu ake pazicitika zoipa . Koma iwo ayenela kuti anadabwa kwambili ataona kuti Petulo mwadzidzidzi waleka kudya nawo . Mwinanso tikuvutika ndi ukalamba ndiponso matenda . Iwo amandithandiza nthawi zonse ndipo ndi zitsanzo zabwino kwa ana anga . ” N’zoona kuti Yesu anali munthu wangwilo ndipo Yehova sayembekezela kuti titengele Mwana wake mwangwilo . Koma kumbukilani kuti Yehova sanamusiye Inoki , ndipo sangasiyenso atumiki ake okhulupilika masiku ano . Koposa zonse , nkhaniyi ndi mbali ya Mau ouzilidwa a Mulungu . Conco ndi yocokela kwa Mulungu wacoodi , “ amene sanganame . ” — Tito 1 : 2 ; 2 Timoteyo 3 : 16 . M’bale wina wa zaka 84 amene mkazi wake anamwalila , anali kuona kuti sangathe kucita upainiya cifukwa ca ukalamba ndi mmene thanzi lake linalili . ( b ) Nanga Aisiraeli akanaonetsa bwanji kuti anali “ anthu oyela kwa Yehova ” ? Cikondi “ cimapilila zinthu zonse , ” ngakhale pamene talakwilidwa , tizunzidwa kapena tikakumana ndi mayeso ena . ( Ŵelengani Oweruza 6 : 23 , 24 ; mau a munsi ) Tikamasinkha - sinkha pa zimene Yehova amaticitila tsiku lililonse , timayamba kumuona monga bwenzi lathu leni - leni . Iwo anagulitsa mbale wao ndi ndalama 20 zasiliva kuti akakhale kapolo . Pa kafuku - fuku winanso anapeza kuti “ kupatsa munthu ndalama kumawonjezela kwambili cimwemwe ca wopatsa ndi wolandila , kuposa ngati azigwilitsila nchito iwo eni . ” Ndipo makhalidwe ena amene kale anali kuonedwa kuti ndi oipa avomelezedwa mwalamulo m’madela ena . Ndipo pa nthawi ina , iye anatsutsa zokamba za anthu odzilungamitsa , amene anali kumunena cifukwa cakuti anali kudya na kumwa . — Luka 7 : 33 - 36 . Coyamba , amatiuza mobweleza - bweleza kuti amafuna kutithandiza . N’ciani cimene lemba la 1 Samueli 8 : 1 - 5 limavumbula ponena za ana a Samueli ? Kukhala ndi mzimu umenewo kumayambitsa mikangano . Koma cimene tidziŵa n’cakuti Mulungu amaseŵenzetsa angelo kuthandiza anthu mwauzimu . Ngati ni woceleza , koma inu muona kuti muliko na vuto pa mbaliyi , ganizilani cimwemwe cimene iye amakhala naco kaamba kothandiza okalamba , odwala , na osauka . M’caka ca utumiki ca 2017 , anthu a “ maganizo abwino ” oposa 284,000 anabatizika poonetsa kudzipeleka kwawo kwa Yehova . ( Mac . A Zimba : Ee , n’zoona . Anthu sakanakwanitsa kupeleka dipo . Kodi inu ndinu citsanzo cabwino kwa acicepele ? Paulo anagogomeza mphoto imene tidzalandila pamene anati : “ Tsopano cifukwa munamasulidwa ku ucimo ndipo munakhala akapolo a Mulungu , mukukhala ndi zipatso za ciyelo , ndipo pa mapeto pake mudzakhala ndi moyo wosatha . ” — Aroma 6 : 22 . 8 : 5 , 14 - 17 ) Ndithudi , Filipo pamodzi na okhulupilila atsopanowo analimbikitsiwa ngako na thandizo limeneli locokela kwa abale a m’bungwe lolamulila ! Anthu ocepa cabe ndiwo anali na makhalidwe abwino monga amene Nowa , Danieli , na Yobu anali nawo , ndipo anaikiwa cizindikilo kuti apulumuke . ( Ezek . ( a ) Ni nkhani ziti zokhudza cilengedwe conse zimene zipezeka m’pemphelo la Yesu ? Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . Baibo inakambilatu kuti anthu ambili ‘ m’masiku otsiliza ’ a dongosolo loipa lino la zinthu , adzakhala odzikonda ndi aumbombo . ( Sal . 83 : 2 - 4 ) Mzele wobadwila mbeu ya mkazi unafunikila kutetezedwa , kuti usaonongedwe ndi kuipitsidwa . Munthu angalonjeze kucita zinthu , kupeleka mphatso , kuyamba utumiki , kapena kupewa kucita zinazake . Kodi tingacite ciani kuti tipindule kwambili na zimene timaŵelenga m’Baibo pa phunzilo laumwini ? M’miyezi yocepa cabe , panakhazikitsiwa kagulu ka mpingo . Zigaŵenga zacikomyunizimu zinali kuyenda - yenda m’midzi n’kumakakamiza anthu kuti aloŵe m’gulu lawo . Komanso akadzaloŵa m’banja , Mulungu adzawathandiza kupeza zosoŵa za mabanja awo . Monga mmene mlimi amaongolela mbeu zimene zapindika cifukwa ca cimphepo , inunso mungathandize abale ena kusintha maganizo kuti ayambe kukalamila maudindo mumpingo . Mulungu anamuuzanso momveka bwino kuti : “ Iye ali m’munda wa mpesa wa Naboti . ” Conco , n’nayamba kucita cidwi ndi zamizimu . ( Luka 11 : 1 , 2 ) Kuonjezela apo , pa ulaliki wake wochuka wa pa phili , Yesu analimbikitsa omvela kuti azipemphela . Takuya anati : “ Ndine n’nali wocimwa , koma Yehova kupitila mwa akulu , anacitapo kanthu kuti anithandize . ” N’cifukwa ninji amuyelekezela ndi “ unsembe wa Melekizedeki ” ? Anali kugwila nchitoyi mwakhama cakuti anali kupeza ndalama zokwanila kuti asamalile banja lao . 1 : 26 - 28 ) Adamu anafunika kugonjela Yehova monga Mlengi wake . Nkhani imeneyi tinaifotokozanso mu Nsanja ya Mlonda ya Cizungu ya May 15 , 1979 , mapeji 30 - 31 . Iwo “ anayankhila pamodzi kuti : “ Mau onse amene Yehova wanena tidzacita . ’ ” ( Eks . Mwacionekele Yesu anadziŵa kuti io anali kuganiza za kacisi weniweni , “ komatu iye anali kunena za kacisi wa thupi lake . ” Ndiyeno , Yehova anauza Baruki kuti : “ Taona ! Ndipo “ mau akewo amathamanga kwambili ” m’lingalilo lakuti nthawi zonse Mulungu amatipatsa mwamsanga malangizo amene timafunikila . Kupemphela kwa “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse ” kungatipatse mpumulo waukulu . Tinafunika kuphunzila cineneloco kuti tizikwanitsa kucititsa maphunzilo a Baibulo ambili amene tinayambitsa . Conco , tinapitilizabe kuyesayesa . Kwa wiki imodzi , yesani kuona mmene mumakambila na mmene mucitila zinthu ndi mnzanu wa m’cikwati . Yambitsani phunzilo la Baibulo pa mpata uliwonse umene mungapeze . Cifukwa amaona kuti ngati zimenezi zingatheke , ndiye kuti anthu sangafunikile kutsogoleledwa na Mulungu , ndipo angakhale na ufulu wocita zilizonse zimene afuna . ( b ) Kodi Yosefe anali na mwayi wotani pamene anali m’ndende ? Conco , tiyeni tiziyesetsa kuthetsa nkhani zaconco mogwilizana ndi mfundo za m’Baibo . Makolo ena amene anasamukila m’dziko lina angaphunzile citundu catsopano ca ana awo , koma osafika pocikamba bwino - bwino . Hutter anafalitsanso Baibo yochedwa Cipangano Catsopano , ndipo inali na zitundu 12 . ( Yesaya 1 : 15 ) Zimenezi zionetsa kuti anthu amene amaphwanya malamulo a Mulungu kapena amene amapemphela ndi zolinga zoipa , mapemphelo ao sangayankhidwe . — Miyambo 28 : 9 ; Yakobo 4 : 3 . Komabe acibale a akazi ao si Mboni , ndipo anafuna kucita miyambo ina yosakondweletsa Mulungu poika malilo . ( 2 Tim . 2 : 20 , 21 ) Ndiyeno , Paulo analimbikitsa Akristu ‘ kupewa ’ kapena kuzipatula ku ziwiya za ‘ nchito yonyozeka . ’ Kulambila kwa pabanja kumathandiza acinyamata ndi acikulile kuti azikondana kwambili ( Onani ndime 12 ndi 15 ) Akatelo , amayamba kudziŵika kuti ndi banja , ndipo cikwati cawo cimafunika kukhala mgwilizano wa moyo wonse . ( Gen . Iwo anazindikila kuti atsogoleli a maiko ao anawapusitsa , atsogoleli a machalichi ao anawanamiza ndipo akulu - akulu a asilikali anawacitila cinyengo . Kukhala wofunika kwa iye , sikumadalila pa kuculuka kwa zimene timacita . “ Kulibe milungu , kulibenso colinga ca moyo . 20 : 35 . [ Mau apansi ] Nkhaniyi idzafotokoza mmene lemba la caka ca 2017 , ingatilimbikitsile kuyang’ana kwa Yehova kuti atithandize pokumana ndi mavuto . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Woyang’ana mphepo sadzabzala mbewu , ndipo woyang’ana mitambo sadzakolola . ” — Mlaliki 11 : 4 . ( Mat . 10 : 23 ) Munthu akathaŵa kwawo , amakumana ndi mavuto mosasamala kanthu za cifukwa cimene wathaŵila . ( Mat . 25 : 21 , 23 ) Kodi Ambuye wathu , Yesu , adzacita ciani akadzabwela mtsogolo ? N’zoona kuti kukhala pabanja ndi kubala ana kumakhala na mavuto ake . Komabe , ngati munthu amafunitsitsa kubala koma sizitheka , imakhalanso “ nsautso m’thupi . ” ( Miy . Kuti tiyankhe mafunso amenewa , tiyenela kukumbukila mitundu ya ziukikilo imene Baibo inalosela . Conco , iye anakana udindo ndi mwai umene akanakhala nao cifukwa cokhala m’banja la Farao . M’kupita kwa nthawi , anzanga ena a m’kilasi monga Larry Androsoff , Norman Dittrick ndi Emil Schneider anaphunzila coonadi , ndipo akutumikilabe Yehova mokhulupilika . Analemba kuti : “ Pa cithunzi cina panali mmbulu ndi mwana wa nkhosa , mwana wa mbuzi na nyalugwe , mwana wa ng’ombe na mkango , zonse zili pamtendele . Ndipo mwana wamng’ono ndiye anali kuzitsogolela . . . . Koma mavuto amene timaona ndi umboni winanso wakuti Satana watsala ndi kanthawi kocepa . N’zoona kuti m’busayo anali wokongola ngati “ mbawala , ” zala zake zinali zolimba ngati “ zagolide , ” miyendo yake inali yokongola ndi yolimba “ ngati zipilala zamiyala ya mabo . ” ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Kodi Elisa anacita ciani cimene cinapangitsa kuti aneneli anzake ayambe kumudalila ? ( 2 Maf . 22 : 8 ; 23 : 2 , 3 , 12 - 15 , 24 , 25 ) Ana ake anali ndi colowa cakuuzimu cabwino kwambili cakuti m’kupita kwa nthawi , ana ake aamuna atatu ndi mdzukulu wake mmodzi anadzakhala mafumu . ( a ) Kodi Baibulo limafanana bwanji ndi galasi ? N’zocititsa cidwi kuti nthawi iliyonse pamene Yehova anaukitsa munthu wakufa , panaliko mtumiki wokhulupilika wa Mulungu , monga Eliya , Yesu , ndi Petulo . Amaopa kuti anthu adzaleka kuwatamanda pa zimene zicitika . ( Aheb . 4 : 16a ) Yehova anatipatsa mwayi wopemphela kwa iye kupitila mwa Mwana wake , amene “ kudzela mwa iye , tili ndi ufulu wa kulankhula ndiponso njila yofikila Mulungu popanda kukayikila pokhala ndi cikhulupililo mwa Yesuyo . ” ( Aef . 1 : 28 . Iyayi , sanacite nkhanza , ndipo Yobu nayenso sanaganize conco . Kuwonjezela apo , ponena za Malemba Aciheberi , katswili wina dzina lake William Henry Green anati : “ Tingakambe motsimikiza kuti palibe zolemba zina zakale zimene uthenga wake unakopedwa mosamala kwambili kupambana Malemba Aciheberi . ” Davide sanangozithamangitsila kutali zilombozo , koma anayamba kulimbana nazo kuti ateteze nkhosa za atate ŵake . Kulankhula ndi mphatso yocokela kwa Mulungu . Kodi mtumwi Paulo anacita ciani pamene anali wacikulile ? Nehemiya atamva za mavuto a anthu ku Yerusalemu , anacondelela Yehova m’pemphelo . ( Neh . Banjali linali litangobwelako ku Iguputo . Ndipo ndi anthu ocepa amene amasangalala kugwila nchito imene saidziŵa bwino . Sitiyembekezela Yehova kuthetsa mavuto athu mozizwitsa tisanaloŵe m’dziko latsopano . Mwacizoloŵezi , akuona mwamuna wake akutulukila capatali kumtunda , ndipo nkhope yake yokongola ikumwetulila . Koma ine ndidzawauza momveka bwino kuti : ‘ Sindikukudziŵani ngakhale pang’ono ! Nikhulupilila kuti Yehova anaseŵenzetsa mnzanga ameneyu kuti anitonthoze . ” Ndipo anatsatila malangizo amenewo mosamalitsa . Mu 1929 , mipingo ya ku Queensland ndi ku Western Australia inakonza makalavani kuti ikwanitse kulalikila kumadela akutali . Mwa thandizo la Yehova , pang’ono m’pang’ono Petulo anayamba kuganiza mofanana ndi Khristu . M’bale wina amakumbukila kuti pa nkhani imodzi ya m’Baibulo amakwanitsa kuphunzilapo zinthu zambili . Ngati ndinu mkulu , kodi mumapatula nthawi yomvetsela pamene mtumiki wothandiza ayeseza nkhani yake ? Koma anamulonjeza kuti adzamupatsa dzikoli monga colowa cake , ndi ca mbewu yake , ngakhale kuti pa nthawiyo n’kuti alibe mwana . ” ( Mac . Pamene Yesu “ anali kunenedwa zacipongwe , sanabwezele zacipongwe . Mosazengeleza alambili okhulupilika anayenela ‘ kuleka kucita zosalungama . ’ Tiyenela kukhala oleza mtima ndi kukamba ndi anthu panthawi imene angamvetsele 6 : 1 . Pokhala Mboni za Yehova , colinga cathu ndi kulalikila uthenga wabwino kwa anthu ambili mmene tingathele mapeto asanafike . 20 : 13 ; 21 : 22 , 23 ; Sal . ( Ŵelengani Luka 21 : 19 . ) Wolemba Salimo 84 , amene ndi mmodzi wa ana a Kora , anali kutumikila pa kacisi wiki imodzi pa miyezi 6 iliyonse . Iye anali kuona zisa za anamzeze pa kacisi . Popeza kuti kunalibe m’bale wobatizika , alongowo anali kukambilana aŵiliŵili mbali zambili za misonkhano . Mavalidwe athu azigwilizana ndi “ mmene [ anthu ] amene amati amalemekeza Mulungu amayenela kudzikongoletsela . ” Kunkhondo , anthu amacita zinthu zoipa kwambili . Koma kusintha kumakhalapo , ndipo kumaonekela osati cabe mwa ziŵelengelo , koma mwa kuona mmene anthu amene alandila uthenga wa Ufumu amasinthila umunthu wao . — Aroma 12 : 2 ; Aef . Conco , mungacite bwino kuyamba kuiŵelenga . Nkhani ziŵilizi zidzayankha mafunso amenewa . M’zikhalidwe zina , mphatso imene acikulile na acicepele amakonda ni ndalama . Zili conco cifukwa angaiseŵenzetse mmene afunila . ( Aroma 6 : 23 ) Mwacikondi , Mulungu “ anapeleka Mwana wake wobadwa yekha [ Yesu Khristu ] , kuti aliyense wokhulupilila iye asawonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” Yehova amasamalila , kuteteza , na kulangiza mpingo wacikhristu . Pemphelo loyamba analipeleka pamene anali paulendo wautali wa pa sitima wopita ku bwalo la ndeke . Ndipo memba aliyense wa bungwelo sadziona kuti ndi mtsogoleli wa abale anzake , koma monga ‘ wanchito wapakhomo ’ wodyetsedwa ndi kapolo wokhulupilika , ndipo amagonjela ku citsogozo cake . A Inoki : Nkhani imeneyi ikufotokoza zimene mungacite kuti mukhale acimwemwe m’banja lanu . 1 , 2 . ( a ) Ndi malo olambilila ati amene atumiki a Yehova anali kugwilitsila nchito kale ? Malinga n’zimene Mateyu analemba , Yesu anachulakonso za Asaduki . Baibulo silikamba msinkhu kapena zaka zimene munthu ayenela kubatizidwa . M’malo mwake , tidzalimbikitsa khalidwe lofunika kwambili limeneli . Ndiyeno , Yesu anagwilitsila nchito mphamvu zake monga Mfumu kuika “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” ( a ) Ndi uphungu wabwino uti umene Azariya anapatsa Asa ? ( Onani cithunzi - thunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Kodi ulamulilo wa Yehova umatipangitsa bwanji kumuyandikila ? Monga Mboni za Yehova , tifunikila kucitanji kuti tipambane ? ( Ŵelengani Salimo 2 : 11 , 12 . ) Iye anawauza kuti nchitoyi idzacitika kwa nthawi yaitali , mpaka “ m’nyengo ya mapeto a nthawi ino . ” Mulungu afuna kuti ‘ tiziyesetsa kucita zabwino , ’ ‘ tizikonda cabwino , ’ ndipo ‘ tizicita zabwino , ’ kuti ‘ atikomele mtima . ’ Mwacitsanzo , Hegai ndi Sesigazi amene anali kulondela akazi ndi adzakazi a mfumu Ahasiwelo , yemwe amaganizilidwa kuti anali Sasita woyamba , anali ofulidwa . — Esitere 2 : 3 , 14 . Anthu andale kwa nthawi yaitali akhala akufunafuna njila zimene angathetsele mikangano . Kodi fanizo la Yesu la kanjele ka mpilu limatanthauza ciani ? Iye ali ndi Mboni zokwana 8 miliyoni zimene zimauza anthu a mitundu yonse zimene anacitila anthu kale , ndi zimene akuwacitila tsopano . Ngakhale kuti papita nthawi yaitali , tiyenela kukhalabe ndi ciyembekezo cakuti madalitso a Ufumu adzakwanilitsidwa . Ife tifuna kuti tizitsogoleledwa ndi mzimu wa Mulungu osati mzimu wa dziko . Ndi mzimu wake , Yehova watithandiza kumvetsetsa bwino - bwino zimene zili pafupi kucitika . Bukuli limanenanso kuti : “ N’zodabwitsa kuti m’mabwinja a Yeriko anapezamo zakudya zambili . ” — Biblical Archaeology Review . Bungwe Lolamulila limapangila pamodzi zosankha zofunika . Tinaona ciŵelengelo ca ofalitsa ndi ca mipingo cikukwela kwambili m’madela amene tinali kutumikila . A Inoki : Ndayamikila cifukwa condiuza zimenezi . ( Ekisodo 12 : 40 , 41 ) Yelekezani kuti mukuona Sara akutembenuka kuyang’ana uku na uku , kuona kukongola kwa dzikolo komanso nyengo yake yabwino . Koma kodi iye amalimbikitsa ena kucita zinthu zoipa ? 24 : 14 ) Mosakaikila , panthawiyo anthu a Mulungu azidzalengeza uthenga woŵaŵa waciweluzo . Yehova waika m’dzanja lathu Mau ake amoyo amene aonetsa kuti uthenga wathu ndi wodalilika , ndipo umacokeladi kwa iye . Ganizilani zimene zinacitikila mlongo wina . Iye anati : “ N’nali kuona kuti mlongo wina anali kucita nane zinthu ngati kamwana . Conco , kodi tonsefe tiyenela kucita ciani mosasamala kanthu za msinkhu wathu kapena thanzi lathu ? Zaka 40 zimene iye anali m’busa , zinam’thandiza kukulitsa makhalidwe amenewa . 2 : 3 , 4 ) Lelolino , otsatila a Yesu , kuphatikizapo khamu la atumiki a nthawi zonse oposa 1,000,000 , amvela malangizo a Paulo amenewa kulingana ndi mmene zinthu zilili pa umoyo wawo . Mu 2000 , Bungwe Lolamulila linaona kufunika kothandizila magulu a omasulila padziko lonse . Ndipo monga mmene takambila poyamba , anthu masauzande ambili padziko lonse akuphunzila Baibulo ndi colinga ca Mulungu . Yosefe anali kudziŵika ngako monga munthu wacikondi , cakuti abale anam’patsa dzina lakuti “ Baranaba , ” kutanthauza “ Mwana wa Chitonthozo . ” ( Mac . ( Yes . 66 : 8 ) Ziyoni , amene ndi gulu la Yehova la zolengedwa zauzimu , anabala ana auzimu ndi kuwapanga kukhala mtundu . Anthu ena amakumbukilabe macimo amene anacita kale ndipo amakaikila kuti Mulungu anawakhululukila . Mukakumana ndi mavuto , Yehova amafuna kuti muzidzimva otetezeka cifukwa amakukondani kwambili . Munthu akapha mnzake mwangozi , anali kukhalabe na mlandu wa magazi cifukwa ca kupha munthu wosalakwa . ( Gen . 31 Kodi Utumiki Wanu Uli Ngati Mame ? ( Ŵelengani Yesaya 66 : 14 . ) 15 : 4 . Kumeneko , anapitiliza kumasulila Baibo mosamala kuti anthu asadziŵe . Nthawi zambili , Yesu sanali kuyankha om’tsutsa malinga ndi zimene io anali kuganiza . Panthawiyo , Danieli anali atatsala pang’ono kukwanitsa zaka 100 , ndipo masiku a moyo wake anali ku mapeto . Muziika zinthu zofunika kwambili patsogolo . 3 : 1 - 6 ) Adamu na Hava sanali kudziŵa zilizonse zokhudza colengedwa cimeneci . Mukanakhala Bezaleli kapena Oholiabu ndipo mwagwila mwakhama nchito ya luso imeneyo koma ndi anthu ocepa amene akuidziŵa , kodi mukanamva bwanji ? Ana athu amakula bwino ngati timawalimbikitsa ( Onani palagilafu 14 ) Ndinali nditakwatila mkazi amene ndinali kukhala naye , ndipo ndinali nditasiya kale kukoka fodya . Nthawi zina ana athu angakhoza kumatamba zinthu zosayenela ali pafupi na ise ! ” Anakamba conco mayi wina dzina lake Karyn . N’cifukwa ciani makolo afunika kumakamba ndi ana awo za Yehova ? Masiku ano , omasulila mabuku amaloŵetsa mau mwacindunji pa kompyuta . Musayembekezele kuti zonse zikhale m’malo . ( Ŵelengani Salimo 100 : 3 - 5 . ) Inde , mungapambane polimbana ndi Satana . ( Yak . 3 : 17 ) Kuŵelenga Baibulo tsiku lililonse ndi kusinkhasinkha kungatithandize kupewa maganizo oipa . Kodi imwe pacanu , mwatsimikiza mtima kucita ciani kuti muteteze cuma canu cauzimu ? N’cifukwa ciani timakhulupilila kuti Yesu ali moyo ? ( Aroma 14 : 19 ) Izi n’zofunika kwambili makamaka panthawi ya mavuto . 6 , 7 . ( a ) N’cifukwa ciani Nowa anayanjidwa ndi Yehova ? Mutsuo na mkazi wake anali kulila pamene anali kuŵelenga nkhaniyo . Anthu ambili zimawavuta kuthetsa cizoloŵezi cotamba zamalisece . Timapindula tikamaŵelenga ndi kuphunzila zofalitsa zimenezi mwakhama Tiphunzilapo ciani pa fanizo la ‘ nyumba yaikulu ’ ? Kuphunzila kukhala wokhulupilika tsopano , kudzakupindulitsani mukadzakula . NYIMBO : 95 , 97 Kumbukilani zimene Yosefe anacita abale ake atamucitila zinthu zoipa . Anyamata ena a m’gulu la acifwamba amene tinali kudana nawo poyamba , ananimenya , ndipo mtsogoleli wawo ananichaya pamsana ndi kukuwa kuti , “ Dziteteze ! ” Kodi Muyenela Kusintha Maganizo Anu ? ( a ) Kodi dzina la Mulungu timaliyeletsa m’njila ziti ? N’zimenenso Satana amacita . Kodi Davide anacila bwanji mwauzimu ? Akanalingalila kuti ziwathela bwanji . ” — Deut . Kwa zaka zambili , Nowa ndi banja lake anali kukhala pakati pa anthu aciwawa ndi okonda kwambili ciwelewele . Kodi kudzipeleka kumatanthauza ciani ? Ngakhale n’conco , anaganizila anzake amene anapita ku maiko ena , koma mabanja ao anali kucitabe bwino kuuzimu . M’kupita kwa nthawi , abale anga onse anaphunzila Baibo na kukhala Mboni za Yehova . N’ciani cimene tifunika kuganizila pamene tisinkhasinkha zitsanzo za amuna ndi akazi okhulupilika akale ? John Wycliffe ndi anthu ena anali ofunitsitsa kuti Mau a Mulungu afikile munthu aliyense . Tingacite zimenezi mwa kuuza anthu kuti madalitso onse amene tidzalandila m’dziko latsopano adzatheka cifukwa ca kukoma mtima kwa Yehova . 12 : 23 ) Ndiyeno , tingapeleke thandizo malinga ndi zosoŵa zao zenizeni . pangano latsopano . ( a ) Panthawi ya cisautso cacikulu , n’ciani cidzacitikila aliyense amene kale anali wodzozedwa koma n’kukhala wosakhulupilika asanalandile cidindo cotsiliza ? Nthawi zina , zimenezi zimaphatikizapo kulangiza mwana kuti asiye khalidwe loipa . ( Akol . 1 : 9 ) Paulo anakambanso kuti : “ Ndikunena zimenezi kuti munthu aliyense asakunyengeni ndi mfundo zokopa . Koma pali enanso ambili amene sakhulupilila angelo olo pang’ono . Yehova amadziŵa zimene tifunikila , ndipo watipatsa cakudya cokwanila kuti tikhale olimba kuuzimu Anandilimbikitsa kuyamba utumiki wa nthawi zonse . Kodi tasintha bwanji mmene timafotokozela nkhani za Baibulo m’kupita kwa nthawi ? Kingsley anali kufunitsitsa kupezeka pamisonkhano , koma zinali zovuta kwambili . Koma pali pano , pamene tikupilila mavuto na mayeselo m’dziko loipali , tiyeni nthawi zonse tizikumbukila kuti dzikoli na ulemelelo umene limapeleka , zikupita . ( 1 Yoh . Cifukwa mau a conco amakhala “ olasa ngati lupanga . ” — Miyambo 12 : 18 . 16 : 1 - 11 ) Iwo anadzinamiza mwa kuganiza kuti Mulungu adzavomeleza kulambila kwao . Ndilinso pa ubwenzi wabwino ndi acibale anga . Ndiye cifukwa cake akatswili ofufuza zinthu zakale anapeza cakudya cocepa m’mabwinja a mizinda ya ku Palesitina imene inagongetsedwa mwa njila imeneyi , ndipo m’mizinda ina sanapezemo cakudya ciliconse . Nkhondoyi inali ciyambi ca nkhondo zoopsa zimene zakhala zikucitika , ndipo zimenezi zapangitsa anthu kugalukila maboma ndi kukaikila atsogoleli ao . Ngakhale n’conco , iye amatidziŵa bwino ndipo amatimvetsetsa kwambili . — Yes . Tonse timafuna kuti Yehova azitipatsa mphamvu kuti tikhalebe olimba pa kulambila kwathu . Mwina umu ni mmene Yohane anadziŵila zocitika za m’mipingo imeneyi . Iye anakamba kuti : “ Anthu akafuna kuniphunzitsa Baibulo , n’nali kukana . Komanso ngati mumalimbana na zilakolako zoipa zakugonana , mufunika kupewa mavidiyo na mawebusaiti osayenela . Kuti nipitilize kukhala na mtendele wa m’maganizo , nthawi zonse n’nali kupemphela , kuimba nyimbo za Ufumu ndi kuganizila mmene nidzalalikilila nikadzamasulidwa . Paulo analembela kalata Akhristu anzake odzozedwa pofuna kuwathandiza kukhalabe okhulupilika kuti akapeze mphoto . Iye anati : “ Ikani maganizo anu pa zinthu zakumwamba . ” ( Akol . Tumikilani Yehova Popanda Cosokoneza : Tiyenela kuika kulambila Yehova pamalo oyamba , ndi kupewa kuononga nthawi ndi mphamvu zathu pa zinthu zosafunika . Akristu oona sangacite zimenezo . ( Aheb . 4 : 12 ) , Sept . Mwacitsanzo , timamvetsetsa mmene iye waonetsela kuti ni wokonda mtendele komanso cifukwa cake amaona mtendele kukhala wofunika kwambili . “ Ofatsa adzalandila dziko lapansi , ndipo adzasangalala ndi mtendele wochuluka . ” — Salimo 37 : 10 , 11 . 15 : 17 ) M’Baibulo , muli zitsanzo zolimbikitsa za amuna ndi akazi amene anacilimika kuti apeze madalitso a Yehova . Ena a iwo ni Yakobo , Rakele , Yosefe , na Paulo . ( Aroma 7 : 15 ) N’ciani cacititsa kuti zinthu zifike pamenepo ? ( 2 Timoteyo 3 : ​ 14 , 15 ) Pa lembali , liu lakuti ‘ kukhutila ’ likutanthauza “ kukhala wotsimikiza kuti cina cake ndi coonadi . ” ( Ezek . 39 : 11 ) Koma kodi colengedwa cauzimu cingadyedwe ndi “ mbalame zodya nyama , mbalame zamitundumitundu ndi zilombo zakuchile ” ? Nifuna muyambe kuphunzila nane Baibo . ” Pamene Yesu anali padziko lapansi , ayenela kuti anali kukamba Ciheberi . NYIMBO : 122 , 139 Pakuti masiku amene timakhala ndi moyo amatha mwamsanga ndipo timacoka mofulumila . ” — Salimo 90 : 10 . 5 : 3 - 5 . ( Onani bokosi la mutu wakuti , “ Kumvetsa Fanizo la Matalente ” ) * Ziyenela kuti zinali zovuta kwa Yesu wacifundoyo , amene mwina anali na zaka 20 kapena kucepelapo , kupilila imfa ya atate ake . Ayenelanso kuti anavutika kwambili poona cisoni cimene amayi ake , azilongosi ake , ndi abale ake anali naco . Kuti zimenezi zitheke , pophunzila sitifunika cabe kuganizila mmene mfundozo zikhudzila anthu ena , koma tiyenela kuganizilanso mmene zikhudzila ifeyo patekha . ( Afil . Kapena angaope cifukwa coganiza kuti sangakwanitse kusamalila udindo . N’cifukwa ciani n’koyenela kusintha kamvedwe kathu ka ukapolo kwa Babulo wamakono ? Kukamba zoona , ngati Yesu anali kufuna kuti otsatila ake azikondwelela tsiku lake la kubadwa , akanaonetsetsa kuti iwo adziŵa bwino - bwino tsiku limene iye anabadwa . Yehova ndiye Mulungu woona , ndipo tifunika kulambila Iye yekha cabe . — Ŵelengani Chivumbulutso 4 : 11 . Iye anazindikila kuti Yehova ndiye anali kuyendetsa zinthu . Kusintha kumene acita ni umboni wakuti “ mau a Mulungu ndi amoyo ndi amphamvu . ” Komabe , anthu amene amapezeka pamisonkhano ayenela kupewa kudodometsa ena mwa kuvala motailila , kutuma mameseji , kulankhula , kudya kapena kumwa , ndi kucita zinthu zina pamisonkhano . Kodi ubwenzi wanu ndi Yehova ndi wolimba ? ( Ŵelengani Machitidwe 17 : 2 , 3 . ) Timadziŵa zimenezo tikafananitsa fanizoli ndi mafanizo ena aŵili . Mwacitsanzo , iye anauza Aisiraeli kuti : “ Lamulo lililonse ligwile nchito mofanana kwa mbadwa ndi kwa mlendo wokhala pakati panu . ” N’nali kukonda kwambili kuphunzitsa anthu Baibulo cakuti n’naganiza zofunsila Sukulu ya Giliyadi Yophunzitsa Baibulo . Ndipo mdani wanu wamkulu , Satana , akuseŵenzetsa cida coopsa kwambili polimbana nanu . Kucokela pamene anaponyedwa pa dziko lapansi , iye wakhala akudziŵa kuti “ wangotsala ndi kanthawi kocepa . ” Atalandila thandizo , iye anati : “ Sindingathe kufotokoza bwinobwino mmene ndikumvela . . . 1 TIMOTEYO 4 : 8 Iwo apitilizabe kutumikila Yehova cifukwa cakuti amakumbukila cikondi cao coyamba pa iye . Tangokambilanako zitsanzo zocepa cabe zoonetsa mmene kuganizila mfundo za m’Baibo kungatithandizile kupanga zosankha zabwino monga munthu wauzimu . Malinga na mfundo zimenezo , munthu aliyense saloledwa “ kukopela mapikica , mabuku , zizindikilo za gulu lathu , nyimbo , mavidiyo , kapena nkhani za pa webusaiti yathu na kuziika pa intaneti ( kutanthauza pa webusaiti ina iliyonse , yotumizilana mafailo , mavidiyo , kapena pa malo ocezela a pa intaneti ) . ” A Zulu : A Zimba , ndikuyamikilani kwambili pa zifukwa ziŵili . N’ciani cina cinali mbali ya colinga ca Mulungu ? Zozizwitsa zimene Yesu anacita zimalimbikitsa a “ khamu lalikulu . ” Iwo amasangalala kukhala ndi ciyembekezo cakuti adzacilitsidwa ku matenda onse . ( Chiv . Koma zimenezo sizoona . Yehova anali kufuna kuti Adamu ndi mkazi wake Hava ‘ abelekane , aculuke , ’ ndi kuti ‘ adzaze dziko lapansi . ’ Yankho : Panafunika wina kuti apeleke nsembe moyo wangwilo wofanana ndi umene Adamu anali nao . Iye anaganiza kuti akakambilane ndi mlongo amene anamukwiyila . DOKOTA WA ZAMISEMPHA DZINA LAKE , ALEXEI MARNOV ANATI : “ Ku masukulu amene n’naphunzila , anali kuphunzitsa kuti kulibe Mulungu ndiponso kuti zinthu zinacita kusandulika kucokela ku zinthu zina . Dikishonale ina inati : “ Kubyala namsongole m’munda wa munthu wina pofuna kumukhaulitsa . . . unali mlandu malinga ndi malamulo a Aroma . Kuti anthu onse a njala ya coonadi apindule , mu August 1914 , Ophunzila Baibulo anatulutsa “ Seŵelo la Eureka , ” kucokela ku “ Seŵelo la Cilengedwe . ” Koma Mary anapitilizabe kukhala mkazi wabwino ndi kuonetsa makhalidwe acikristu . Nchito yake inali kuteteza Aisiraeli ndi kuwapangila zosankha zabwino . Yehova anatumanso Eliya kuti akapeleke uthenga wina kwa iye . Mdani wanu Mdyelekezi akuyendayenda uku ndi uku ngati mkango wobangula , wofunitsitsa kuti umeze winawake . ” — 1 PET . Nkhani yaciŵili idzatikumbutsa mmene tingapewele kucita zinthu zimene zingatilepheletse kudzalandila madalitso amene Yehova walonjeza . Koma ni okongola kwambili cakuti “ ngakhale Solomo mu ulemelelo wake wonse sanavalepo zokongola ngati lililonse la maluwa amenewa . ” Cinthu cofunika kwambili cimene tingacite ndi kuŵelenga ndi kuphunzila Baibulo nthawi zonse . ( Mac . 11 : 26 ) Paulo anadziŵa kuti n’kofunika kutsatila ziphunzitso zozikidwa pa Baibo zimene atumwi ndi amuna ena otsogolela anali kuphunzitsa . Ndi mwai waukulu kukondedwa ndi Yehova . ( 2 Akorinto 9 : 15 ) N’cifukwa ciani Paulo ananena mau amenewa ? Koma inu cifukwa cophunzila Baibulo , mwadziŵa coonadi ponena za Yehova . Ndipo sanacedwe kukonzela ciwembu Yesu pamene anali mwana . Kodi mungaphunzitse bwanji ana anu kupewa zosangulutsa zoipa ? Mwacidziŵikile , atumwi anaphunzilapo kanthu pa citsanzo ca Yesu ca kukonda “ anthu a mtundu uliwonse . ” ( Yoh . 12 : 32 ; 1 Tim . Ndiko kukoma mtima kosayang’ana nkhope . Iye sanali wakufa monga mmene adani ake anali kuganizila . N’naphunzila kuona zabwino zimene amacita , na kunyalanyaza zofooka zawo . ” Kunena mwacidule , umoyo wake sukuyenda bwino ngati mmene anali kuyembekezela . NYIMBO : 73 , 36 Masiku ano , webusaiti yathu imatithandizanso kulalikila anthu okhala m’madela akutali . 29 Cifukwa Cake Kucotsa Munthu Mumpingo Ndi Makonzedwe Acikondi Muzicita zilizonse zimene mungakwanitse pocilikiza kulambila koona . 3 Kukumbukila Cikondi Canga ca Poyamba Kwandithandiza Kupilila Mavuto na nkhawa za mu umoyo zingatipanikize ndi kucititsa manja athu ophiphilitsa kulefuka . Conco , anatenga “ galeta lokokedwa ndi mahachi , ndipo amuna 50 anali kuthamanga patsogolo pake . ” Pamene mkambiyo akamba nkhani yake , akuyenda uku na uku pa pulatifomu , kwinaku akucita magesica . Iye akulumikiza malemba na kuwafotokoza mwaluso cakuti mwamuna wacidwi uja wayamba kumvetsetsa coonadi ca m’Baibo . Conco , cifukwa cacikulu cimene Yehova , kupitila mwa Yesu , anatimasulila ku ukapolo wa cilamulo ca ucimo na imfa n’cakuti tidzipeleke kwa Mulungu “ monga akapolo ” ake . 17 : 16 . Ciliconse cimene cili m’dziko lapansi cimapindulitsa anthu ndi nyama . Ife anthu tikaona malo okongola m’mabuku , m’magazini , kapena pa TV , timafuna kuyenda kumalo amenewo a “ paradaiso ” kukasangalala ndi kuiŵalako mavuto athu . Pamene tinabatizika , tinaonetsa poyela kuti tsopano ndise a Yehova komanso kuti ndise ofunitsitsa kumumvela . ( Aheb . 12 : 9 ) Izi n’zimene Yesu anacita . M’nthawi za Baibulo , amuna ena anali kufulidwa monga mbali ya cilango , ndipo ena anali kufulidwa akagwilidwa monga akapolo . Ndinayamba kudziŵika ndi mbili yoipa kwambili ndipo posapita nthawi ndinaitanidwa kuti ndikhale m’gulu la zigaŵenga . Amacita izi , uku akukulimbikitsani kuti : “ Usacite mantha . Komabe , kodi timakhulupililadi kuti Ufumu ndi weniweni ndi kuti udzakwanilitsa cifunilo ca Mulungu ? M’nkhani yapita , tinaphunzila mmene ife anthu ocimwa timapindulila ndi kukoma mtima kwakukulu kumene Yehova amaonetsa m’njila zambili . Kodi tiyenela kuuona bwanji udindo wopanga zosankha ? Mu July 1984 , ndinatumizidwa ku ndende ya Dzaleka kumene kunali Mboni zina 81 . Uwu ni ufulu waukulu kwambili . Ndipo munthu angakhale na ufulu umenewu olo pamene ali m’jele . ( Gen . Tinabwela kuno kuti tithandize anthu , koma taona kuti zocitika za kuno zatithandiza kwambili . Muyenelanso kupewa kukhala aŵiliŵili pa malo obisika . Kingsley ndi Paul ( Ŵelengani Mateyu 4 : 23 , 24 ; Yohane 9 : 1 - 7 ) Tikamaganizila zozizwitsa zimenezi , timayembekezela mwacidwi zinthu zosangalatsa zimene Yesu adzacita m’dziko latsopano . Aroma 8 : 15 , 16 ; 1 Yohane 2 : 20 , 27 Mwacitsanzo , mukaona namzeze , muzikumbukila kuyamikila nyumba yolambililamo Yehova . Cimene cimanikondweletsa ngako n’cakuti kubwela kuno kwathandiza kuti ana anga apitilize kucita utumiki wopindulitsa kuno . ” ( 1 Sam . 25 : 32 ) Nabala atafa Davide anakwatila Abigayeli . — 1 Sam . Kodi zitsanzo za Yehova , Yesu , na mtumwi Paulo zimatiphunzitsanji pa nkhani yolimbikitsa ena ? Ni mfundo ziti zokhudza dipo zimene tingagogomeze ? ( 2 Pet . 2 : 9 ) Tili ndi zifukwa zabwino zodalila Yehova , ndi kupitiliza kupilila mayeselo molimba mtima . Cakumapeto kwa zaka za m’ma 1800 , atumiki a Yehova anayamba kumvetsetsa tanthauzo la ulosi wa Danieli umene analemba zaka zoposa 2,500 zapitazo . Ulosi umenewo umati : “ M’masiku a mafumu amenewo , Mulungu wakumwamba adzakhazikitsa ufumu umene sudzawonongedwa ku nthawi zonse . ” ( Dan . wopatsa ? ) Kodi Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lokonzedwanso la cingelezi ndi labwino motani ? Kodi pali mkazi wamasiye amene afuna kuti wina akamuthandize kukonza nyumba yake ? Tikakhala anthu auzimu , tidzakhala na umoyo wacimwemwe lomba ndi ‘ moyo weniweni ’ mtsogolo . — 1 Tim . Ndi ubwenzi wotani umene unalipo poyamba pakati pa Aiguputo ndi mbadwa za Yakobo ? Tiphunzilapo ciani pa mau akuti “ Atate wathu ” ? Yesu analinso kuzindikila makhalidwe abwino a ophunzila ake . Kuti tithandize anthu kupeza mayankho , timagwilitsila nchito buku lakuti , Zimene Baibo Imaphunzitsa . ( Chivumbulutso 3 : 19 ) Mwacitsanzo , nthawi zambili ophunzila ake anali kukangana za amene anali wamkulu pakati pao . ( Afilipi 4 : 6 , 7 ) Inde , mukhoza kum’pempha Yehova kuti akupatseni mtendele . Kodi ciyembekezo cimatithandiza bwanji kucepetsa nkhawa ? Satana adzaonongedwa kothelatu ( Onani ndime 18 ) Pamene n’nali na zaka 7 , ananidula manja kucipatala kuti apulumutse moyo wanga . Iye anati : “ Ndikalibe kubwela ku Russia ndinali mkulu ndiponso mpainiya koma tsopano ndikuona kuti ubwenzi wanga ndi Yehova walimba kwambili . ( b ) Kodi makolo angathandize bwanji ana ao kukhala okhulupilika akakumana ndi ziyeso ? Iye anamva conco ngakhale kuti anali kudziŵa kuti adzaukitsa Lazalo . Khalani ndi Cikhulupililo Cosagwedela mu Ufumu Ophunzila Baibo anazindikila kuti sizinali zokwanila kungodziŵitsa cabe abululu ŵawo , anzawo , na mamemba a chechi yawo zakuti acoka m’cipembedzo conama . Ndiyeno , kumeneko mwapeza anthu , zikhalidwe , zakudya , ndi ndalama zimene inu simunazionepo . Baibo imakambanso kuti : “ Mtima wosangalala ndiwo mankhwala ocilitsa . ” Nanga mungacite ciani ngati mau anu amamveka ofooka kapena okwela kwambili ? Mulimonse mmene zinalili , iwo anacoka ku Harana na kupitiliza ulendo . Mabanja ambili amagaŵa nthawi ya kulambila kwa pabanja m’zigawo zingapo . Pamene Yehova anam’sankha kuti akadzudzule Ufumu wa mafuko 10 wa Aisiraeli kuti aleke kulambila mafano , Aisiraeli ena ayenela kuti anaona kuti Mulungu sanasankhe bwino . — Ŵelengani Amosi 7 : 14 , 15 . Conco , tisapatse munthu wina udindo wotipangila zosankha . Mwacitsanzo , bwanji ngati mufuna kuleka sukulu yasekondale cifukwa cakuti mwatopa nayo ndipo mufuna kuyamba upainiya ? Mose anadziŵa kuti kucita zimenezi kunali kovuta , ndi kuti ‘ akanatonzedwa . ’ Mwadzidzidzi , asilikali a Roma anacoka ndipo zimenezi zinapatsa otsatila a Yesu mpata wakuti acoke mu Yerusalemu ndi mu Yudeya . Ngati n’telo , musaope kupanga lonjezo limenelo . NYIMBO : 72 , 119 Mulungu wakhala akulamulila monga mfumu kwa zaka zambili kuposa munthu wina aliyense . Tiyeni tikambilane citsanzo ndi kuona mmene tingapangile zosankha mwanzelu ngati tiganizila zimene Yehova afuna . Koma Satana amagwilitsila nchito mphamvu zake molakwika . 10 : 24 . “ Limbani m’Cikhulupililo ” Baibulo limati : “ Ahabu atangomva mau amenewa , anang’amba zovala zake n’kuvala ciguduli . Iye anayamba kusala kudya , kugona paciguduli ndipo anali kuyenda mwacisoni . ” Zinali kunivuta cakuti n’taphunzilako maulendo oŵelengeka , n’naleka . Zotulukapo zake , iwo sakhumudwa kapena kutaya mtima na mavuto amene amakumana nawo . Kupanda ungwilo kwathu kungatisonkhezele kucita zinthu zoipa . N’zosangalatsa kwambili kuona mmene Yehova akumveketsela bwino coonadi . Anthu amada nkhawa kwambili ndi zosoŵa zao , zooneka ndi zosaoneka zomwe , ndipo amafunafuna zinthu zosafunika kwenikweni . Nthawi ya cikwati cimeneci yayandikila kwambili . Ngakhale akulu odziŵa bwino nchito yao ayenela kukumbukila kuti mtsogolo adzalephela kusamalila maudindo ena mumpingo cifukwa ca ukalamba . Lembali silifotokoza cifukwa cake . Mwacionekele , umu ni mmenenso Adamu na Hava anali kumvelela . tikhale na makhalidwe abwino kwambili ? Rabeka anali kugwila nchito mwakhama ndipo anali woceleza Kupanga zosankha . Kunena zoona , munthu akamakalamba amafunika kusintha zinthu zina ndi zina . ( Akolose 3 : 14 ) Koma kodi Yesu anali kungofuna kugwilizanitsa anthu a zikhalidwe zosiyana - siyana kuti azikhala mwamtendele ? Baibulo silikamba nthawi imene Luka anaphunzila za udokotala kapena kumene anaphunzilila . Yesu Kristu anali kuwadziŵa bwino Malemba ndi kuwamvetsetsa . [ 1 ] ( palagilafu 14 ) Pali zolinganako zambili pakati pa ukapolo wa Ayuda wa zaka 70 ku Babulo , na zimene zinacitika kwa Akhiristu mpatuko utayamba . Mofanana ndi Akhristu ena onse , othaŵa kwawo amafunika kupewa mzimu wokonda zinthu zakuthupi kuti asawononge ubale wawo na Yehova . Yesu anati : “ Cotelo pitilizani kufunafuna ufumu coyamba ndi cilungamo cake , ndipo zina zonsezi zidzawonjezedwa kwa inu . ” ( Mat . Motelo , tili ndi zifukwa zomveka zokhulupilila kuti Yehova amadziŵa bwino zimene tingakwanitse kupilila . Yehova ndiye anapanga kumwamba ndi dziko lapansi ndipo ndiye Wolamulila cilengedwe conse . Pezani malo abwino . Kuonjezela pamenepo , ulamulilo wa Yesu udzakhalapo “ mpaka kalekale , ndithu mpaka muyaya . ” Yosefe wacinyamatayo anadziŵa kuti palibe ciliconse cimene angacite ndipo sadzaonananso ndi atate ake okalamba . Lemba la caka ca 2018 n’lakuti : “ Anthu odalila Yehova adzapezanso mphamvu . ” — Yes . Nanga tingakonzekele bwanji Cikumbutso ? Yesu anatiphunzitsa kuti nthawi zonse tiyenela kukhala okonzeka kukhululukila ena . — Mateyu 6 : 14 , 15 ; 18 : 21 , 22 . Kulalikila kumalo amene kukufunika ofalitsa Ufumu ambili kumacititsa munthu kukhala ndi umoyo wosangalatsa kwambili . ” Kodi mungacite ciani ngati zotele zacitika masiku ano ? Kaya tili m’banja kapena ai tifunika kupewelatu ciwelewele ca mtundu uliwonse . Mlongoyo anapitiliza kuti : “ Nkhani imeneyo inan’thandiza kuona ubwino waukulu wa Yehova . ( b ) Kodi makolo angatani kuti ana ao ayambenso kuwakonda ? N’zoona kuti amacita zimenezi ndi zolinga zabwino . ‘ Anaona ’ Malonjezo a Mulungu Michael mmodzi wa io anati : “ Papita zaka zambili pamene tinacitapo ulaliki umenewu , conco tinali ndi mantha kwambili . ( Ŵelengani Chivumbulutso 4 : 11 . ) Mwacitsanzo , nthawi ina anthu ena sanamvetsetse zimene Yesu anali kuwaphunzitsa . Tiyenela kulimbikila kucita ciani kuti tipeze madalitso a Yehova , potengela citsanzo ca Yakobo , Rakele , ndi Yosefe ? Iye anati : “ Nimakonda kulalikila uthenga wabwino cifukwa n’zimene Yehova afuna kuti tizicita . “ Yoswa mwana wa Nuni anali wodzazidwa ndi mzimu wa nzelu . ” ( Deut . Nyimbozi ni mbali ya cakudya cauzimu cokonzewa na “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” — Mat . Buku la Chivumbulutso limafotokoza zambili pankhaniyi , ndipo limaonetsa kuti masoka amene akucitika padzikoli ali kaamba ka nkhondo imene inacitika kumwamba . — Onani bokosi lakuti “ Nkhondo Kumwamba ndi Padziko Lapansi . ” Koma kodi timaona kuti umenewu ni mwayi woonjezela utumiki wathu kwa Mulungu ? Ngakhale Yohane ndi mtumwi Paulo , amene anali kutsogolela mumpingo , anatsutsidwa . Kodi ophunzila a Yesu analalikila uthenga wabwino kufika pamlingo wotani ? Anazindikilanso kuti mwanayo anayamba kukonda kwambili zinthu zakuthupi osati za kuuzimu ndi banja lake . Kutaca , anayamba kusakila zofalitsa zimene zikanawalimbikitsa mwauzimu . 2 : 4 ) Cikondi cimeneci candithandiza kuti ndisamangoganizila zinthu zoipa zimene ndinaona kunkhondo ndiponso candithandiza kupilila mavuto ena . — Yes . ( Ŵelengani 1 Akorinto 11 : 27 - 34 . ) Ngati Mulungu sachulidwa mumgwilizano wao , kodi ungakhale wothandiza ? Zilembo zinayi zaciheberi zoimila dzina lopatulika la Mulungu lakuti Yehova , zinali kuŵelengedwa kucokela kulamanja kupita kumanzele Mavuto amene Nowa anakumana nawo . Pang’onopang’ono , Alan akumvetsa mmene m’bale wacikulileyo amamvelela cifukwa colephela kuŵelenga Baibulo kapena kulalikila kunyumba ndi nyumba . M’bale Poggensee komanso abale ena ambili okhulupilika monga iye , analeka kudya zizindikilo , koma anapitiliza kupezeka pa Cikumbutso . Ngati sindise oleza mtima , cikondi cathu kwa anthu ena cimacepa . Popeza malamulo amasiyana malinga ndi dziko , muyenela kufunsanso anthu odziŵa bwino za malamulo na misonkho . 28 kutanthauza kuti “ N’ciani ici ? ” Panalinso zambili zimene anali kufunika kucita mu mpingo . Tiyeni tione mmene amapindulila . 5 : 19 , 20 . ( Mac . 5 : 42 ; 6 : 7 ) Akristu ena , monga Filipo , anagwila nchito yaumishonale ku Palestine . ( Mac . Mau akuti “ wamoyo ” anamasulidwa kucokela ku liu la Ciheberi lakuti ne’phesh , limene limatanthauza “ colengedwa copuma . ” — Genesis 2 : 7 , nwt - E mau amunsi . ( Mat . 22 : 38 , 39 ) Yesu anakambanso kuti kukondana cidzakhala cizindikilo ca Akhristu oona . Zikatelo , wolakwilidwa ayenela kukhululukila m’bale wake kuti akhale nayenso pamtendele . Kukamba zoona , ku Nyumba ya Ufumu abale ndi alongo anandionetsa cikondi mwa kumwetulila kusiyana ndi anthu ena amene anali kukhalila kundiyang’ana . Wokwelapo wake dzina lake linali Wokhulupilika ndi Woona . ” M’bale Pierce anali wakhama kwambili potumikila Yehova cakuti anali kudzuka m’mamaŵa , ndipo nthawi zambili anali kugwila nchito mpaka usiku . Iye anafika pa msinkhu wakuti sangabeleke . Sanakhutile ndi madalitso akuti : “ Mubelekane , muculuke , mudzaze dziko lapansi , ndipo muliyang’anile . ( Luka 7 : 11 - 15 ) Panthawi ina Yesu anaukitsa kamtsikana ka zaka 12 . 15 : 2 - 4 ; 16 : 16 ; 21 : 5 . Kodi n’ciani cinathandiza Dokotala ameneyo kuleka kukoka ? Umu ni mmenenso zimakhalila na anthu amene aphunzila za Yehova ali aakulu kale . Muzilalikila uthenga wabwino ( 1 Akorinto 11 : 23 - 26 ) Tonse timasonkhana pa tsiku limodzi , pa Nisani 14 , dzuŵa litangoloŵa poonetsa kuyamikila zinthu zimene Yehova waticitila ndi kumvela lamulo la Yesu . Cotsatila , anakamba bodza lamkunkhuniza kuti : “ Kufa simudzafa ayi . ” Iye anaonetsanso maganizo a Yehova kwa anthuwo pamene anati , “ mwana wa cionongeko . ” Kodi lemba la Zekariya 6 : 15 likukwanilitsidwa bwanji masiku ano ? N’cifukwa ciani takamba zimenezi ? Tiyeni tikambilane zitsanzo ziŵili za anthu amenewa . Iye anazindikila zimene Baibo imakamba ponena za kuthambo na dziko lapansi . Imati : “ Ndipo zonsezi zidzatha ngati covala . ” Ngakhale masiku ano , anthu ena amaumba zinthu zokongola kwambili ndi manja awo . Mwina iye ndiye anapeleka mkanjo wodula wopanda msoko umene Yesu anali kuvala . Muziŵelenga Mau a Mulungu mwakhama , na kuŵasinkha - sinkha Izi zinalimbitsa kwambili cikhulupililo canga , na kunicititsa kukhala wofunitsitsa kufalitsa coonadi ca m’Mau a Mulungu . Kumbukilani kuti misonkhano yonse ya mpingo ni mbali ya kulambila kwathu . Kaini anadzibweletsela mavuto aakulu amene akanatha kuwapewa . ( Gen . 4 : 11 , 12 ) Ha ! COSANKHA COFUNIKA KWAMBILI CIMENE MUNGAPANGE Nkhani yotsatila idzaonetsa mmene tingacitile zimenezi . Ngati tikonda Ufumu wa Mulungu monga mmene wamalonda anakondela ngale , kodi tidzacita ciani ? 5 , 6 . ( a ) Kodi Yesu anaphunzitsa kuti n’ciani cingatithandize kukhala acimwemwe ndi otetezeka ? ( Oweruza 5 : 8 ) Yehova anapeleka Aisiraeli m’manja mwa adani ao , cifukwa anayamba kutumikila milungu ina . Kodi mafanizo amene Yesu anakamba onena za wamalonda woyendayenda ndi cuma cobisika amatanthauza ciani ? Kodi mumayelekezela kuti muli m’dziko latsopano ? Kodi Yehova wapeleka citsanzo canji pa nkhani ya kudziletsa ? Pa nthawiyo , ma IUD amene anali ofala anali tuzipangizo twapulasitiki tumene anali kutuika m’cibalilo n’colinga cakuti mkazi asatenge mimba . “ Mwanawe . ” Ife tidziŵa kuti tili mkati mweni - mweni mwa “ nthawi yamapeto , ” ndipo “ cisautso cacikulu ” cidzayamba lomba apa . ( Dan . Pambuyo pake anawalandilanso pamene anaukitsidwa . Ndiyeno , anakambanso za anthu amene “ sanalole kusiya cikhulupililo cawo kuti amasulidwe . Tikutelo cifukwa cakuti palibe munthu amene akhoza kudziŵa Akristu amene adzalandiladi mphoto yao . Abale ambili analibe magalimoto , conco palibe amene anali kubwela kudzanditenga ku sitesheni ya sitima . Iwo anali atapanga malamulo akuti munthu akalibe kudya , anali kufunika kusambitsidwa manja mpaka ca m’mapewa . Nanga amene amadzipeleka mofunitsitsa kukatumikila kumalo osoŵa amapeza mapindu ena ati ? Nimakwanitsa kudziŵa kuti anzanga eni - eni ni ati , mwa kuona mmene iwo amacitila zinthu komanso mmene ine nimamasukila nikakhala pakati pawo . ” — Courtney . Kwa zaka mahandeledi ambili , iye anali kuwatsogolela ndi malamulo ake . Popeleka ciweluzo , jaji amene anali kuweluza mlandu wawo anati : “ Cipembedzo cimene amuna awa alimo n’coopsa kwambili kupambana gulu la asilikali acijelemani . . . Ndiyeno , anandipempha kuphunzila Baibulo . Pasanapite nthawi , ndinazindikila kuti kudziŵa Yehova ndi colinga cake n’kofunika kwambili kuposa msinkhu wanga . Anthu ena amaganiza kuti kupemphela n’kutaya nthawi ndipo palibe amene amamvetsela . Ganizilani zimene zinacitika pamene mphepo yamkuntho yocedwa Sandy inakuntha mzinda wa New York mu October 2012 . Conco , cimasulilo ca liulo cakuti “ kukoma mtima kwakukulu , ” mu Baibulo la Dziko Latsopano n’coyenelela . Pambuyo pondandalika malemba angapo osagwila mau , magaziniyo inafotokoza cifukwa cake munthu wopepa fwaka wosalapa ayenela kucotsedwa mumpingo . ( 1 Akor . 5 : 7 ; 2 Akor . M’malomwake , iye anati , “ Ndine wokondwa kwambili cifukwa ca cikondi cimene Yehova amanionetsa tsiku lililonse . ” Kodi nchito ya Nyumba ya Ufumu n’ciani ? Nanga zimenezi ziyenela kukhudza bwanji mmene timaonela misonkhano yathu ? Boazi anacita cidwi na cikondi ca Rute kwa mpongozi wake Naomi . Anacitanso cidwi kuona kuti wakhala mlambili wa Yehova . Apolisi anatilamula kuti ticoke mumzindawo . Anagwila ine , Antonio Tsoukaris , ndi Ilias . Tinawapempha mocondelela kuti asatitenge cifukwa ndife Akhristu ndipo sititengako mbali m’nkhondo . Kodi ulosi wa Danieli wakwanilitsidwa bwanji ? Zimatitetezela pa zinthu zina . ( Mlal . “ Iwo saumilila maganizo awo . Conco , n’naphunzila kusamba mosamala m’kamsasa kapanja . N’naphunzila zambili kwa m’bale wauzimu komanso wokhulupilika ameneyo . Anthu amaona kuti ziphuphu sizingathe , koma Baibulo limaonetsa kuti zinthu zidzasintha ndipo ziphuphu zidzatha . Koma kodi n’ciani cidzatithandiza kucita zimenezi ? Pamene ndinali ndi zaka 17 , makolo anga anabwelela ku Germany . Kodi Mulungu amatonthoza bwanji ? Ndipo kwa zaka zambili , anthu oona mtima anagwila nchito yomasulila ndi kufalitsa Mabaibo mwakhama , ngakhale kuti anakumana ndi mavuto . ( Aheb . 5 : 14 ) Komanso , tidzakwanitsa kupanga zosankha mwanzelu ngati titsatila malangizo a mtumwi Paulo akuti cikondi cathu pa Mulungu siciyenela ‘ kukhala caciphamaso . ’ Yehova analandila nsembe imeneyo , kuti aliyense wokhulupilila mwa Yesu adzakhale ndi moyo wosatha . — Aroma 3 : 23 , 24 ; 1 Yohane 2 : 2 . Alejandro , amene wakhala na umoyo wokuka - kuka , anazindikila kuti pamatenga nthawi kuti munthu ajaile mu mpingo watsopano . N’cimodzimodzinso ndi matenda angafikile wina aliyense panthawi iliyonse . Komabe , zimenezo sizinatanthauze kuti Mulungu sadzakhala ndi gulu la atumiki ake okhulupilika padziko lapansi . Ngati munthu amakonda kudela nkhawa za kutsogolo , angayambe kudzidalila m’malo modalila Yehova . Ndipo kucita zimenezi kungasokoneze unansi wake ndi Yehova . — Miy . Munthu wina amene sakhulupilila kuti kuli Mulungu anaganiza mmene Mulungu alili ndipo anapemphela kuti : “ Ngati muliko , mundiŵeleŵeseko cabe . ” Nthawi na nthawi , iye amaonjezela nkhani imodzi kapena ziŵili pa nkhani zimene anasonkhanitsazo . Abulahamu , amene anali kuchedwa “ tate wa onse . . . okhala ndi cikhulupililo , ” anali mutu wa banja lalikulu . ( Aroma 4 : 11 ; Gen . Ndine wokondwa kuti kucokela nthawi imene n’nakhala Mboni mu 1958 , nakhalabe wokhulupilika pa zosankha zimene n’napanga pa umoyo . Nthawi imeneyo , kagulu ka akulu - akulu a chechi kanayamba kuonekela . mu Nsanja ya Olonda ya October 15 , 2011 , mapeji 9 - 12 , mapalagilafu 6 - 15 . Anthu ena amacita manyazi kufunsa mafunso amenewa . Iwo amaganiza kuti mayankho ake ni ovuta kuŵamvetsa . Zimenezi zacititsa anthu ambili kuganiza kuti kufunafuna cipembedzo coona n’kopanda phindu . Munthu akagwilitsila nchito kacidindo kamene kali patsamba lothela , kadzamtsogolela pa Webusaiti yathu . A Inoki : N’zoona . 5 : 8 , 9 ) Webusaiti yathu imathandizanso kwambili kufalitsa uthenga wabwino ngakhale m’maiko mmene nchito yathu ndi yoletsedwa . Munthu wauzimu ? Cifukwa cakuti Baibulo limalimbikitsa aliyense wa ife ‘ kugwilitsa nchito mphamvu zake za kuzindikila , . . . kusiyanitsa coyenela ndi cosayenela . ’ Conco , sipayenela kucitika cina ciliconse cokhudza malonda . — Yelekezani ndi Nehemiya 13 : 7 , 8 . ( b ) N’ciani cimene Yesu anauza otsatila ake kucita ngati io akuona kuti mapeto akucedwa ? Nili na Robert Wallen , Charles Molohan , ndi Don Adams Kumbukilani fanizo la Yesu limene takambilana m’nkhani yapita . Iye anakamba kuti : “ Cipata colowela ku moyo n’copapatiza komanso msewu wake ndi wopanikiza , ndipo amene akuupeza ndi owelengeka . ” “ Yehova ali pafupi ndi onse . . . amene amamuitana m’coonadi . ” — Salimo 145 : 18 . Mulungu amaseŵenzetsa Ufumu umenewo kuti akwanilitse cifunilo cake kumwamba na padziko lapansi . — Mateyu 6 : 10 . Cifukwa ca maganizo amene aya , anthu ofika mamiliyoni amagwila nchito ma awazi ambili kuti apeze ndalama zoculuka . Panthawiyo , mkulu wanga anali pafupi kutsiliza maphunzilo a ku sekondale , ndipo atate anapempha ahediwo kuti mkulu wangayo na ine tiziyenda ku sukulu pa masiku osiyana . Ngakhale kuti sitingakhale onyada monga Sauli , tiyenela kuyesetsa kupewa zilizonse zimene zingaticititse kukhala osamvela . ( b ) Ndi nkhani zotani zimene zili m’Baibulo ? Mulimonse mmene zinthu zilili paumoyo wanu , citsanzo ca Yobu cingakutonthozeni . Panthawi yochedwa Mtendele wa Aroma ( Pax Romana ) panalibe nkhondo . Ana anu amaphunzila citundu ca m’dziko limene munasamukilako akakhala ku sukulu komanso akakhala ndi anthu ena . Monga mmene zinalili ndi Aisiraeli ku Refidimu , timadalila Mulungu kuti atiteteze tikayanganizana ndi adani . ( Genesis 6 : 11 - 13 ) Kodi mwaona umboni woonetsa kuti ciwawa cikuonjezeka padziko ? Mwacitsanzo , atakwapulidwa koopsa na kuponyewa m’ndende , “ capakati pa usiku , [ iwo ] ” anayamba “ kupemphela ndi kutamanda Mulungu poimba nyimbo . ” ( Mac . 22 : 33 - 40 ) M’malo mosimbila omvela ake nkhani zokhudza umoyo wakumwamba , kapena mmene zinthu zinalengedwela , iye “ anatsegulilatu maganizo awo kuti amvetse tanthauzo la Malemba . ” 60 : 22 ; Hab . 2 : 3 ) Nchito yomangayi ikuphatikizapo kumanga maofesi a nthambi , Nyumba za Misonkhano , Nyumba za Ufumu , Maofesi a Omasulila Mabuku , ndi nyumba za masukulu ophunzitsa atumiki m’maiko ambili . “ Ndidzakupatsani malangizo abwino . ” — MIY . ( b ) N’cifukwa ciani sitiyenela kutaya mtima ngati tacita colakwa mobweleza - bweleza ? Mwana wake amene ali ndi zaka 20 , tsopano ndi m’bale wobatizidwa . 5 : 23 , 24 ) Imaticenjeza mwamphamvu kuti sitifunika kuleka kugwilizana ndi mpingo . Mwacitsanzo , mumafunika kuphunzitsa ana anu kumvela lamulo la m’Baibo lakuti : “ Uzilemekeza bambo ako ndi mayi ako . ” ( Aef . KUKULA KWANGA : Ndinakulila ku Rmaysh , ku malile a Israel ndi Lebanon . Nthawi imeneyi n’kuti nkhondo ya pa ciweniweni ili mkati . DZIKO : AUSTRALIA Mkristu wofikapo amalimbikitsa mgwilizano mumpingo . ( Onani bokosi yakuti “ Zimene Tiphunzilapo , Osati Zimene Inali Kuimila . ” ) Ndipo zimene tingakambe zingawalimbikitse . 8 - 12 . Mpaka lelo , ndife mabwenzi apamtima . M’malo mwake , tiyenela kuzindikila zimene Yehova amafuna ndi kucita zimene zimam’kondweletsa . Kodi izi zinawathandiza bwanji ophunzila ? Nthawi ina ali kumeneko anagwidwa . ( Ŵelengani Genesis 39 : 7 - 9 . ) Muzicita zimene mwakamba . Iye anaika maganizo ake pa kucita cifunilo ca Mulungu , cimene ndi kupeleka moyo wake nsembe . Ngakhale kuti limakamba zoona pa nkhani zakale , ndimaona kuti lilibe phindu kwenikweni masiku ano . Koma ngati mumapemphela nao pamodzi , ana anu angaphunzile kudalila Yehova . M’caka ca 1927 , nchito yolalikila kunyumba ndi nyumba pa Sondo inalinganizidwa . Yehova anam’lonjeza kuti adzakhala ndi mwana , koma panapita zaka zambili kuti iye ndi mkazi wake Sara akhale ndi ana . Pokamba za madalitso onse amene Mulungu adzapatsa alambili ake kupitila mwa Yesu Khristu , Paulo anati : “ Tikuyamika Mulungu cifukwa ca mphatso yake yaulele , imene sitingathe n’komwe kuifotokoza . ” Kuonjezela pamenepa , mitu ya nkhani sinalembedwe pamwamba pa masamba , koma inalembedwa monga tumitu tung’onotung’ono mkati mwa nkhani kuti anthu asamavutike kupeza mfundo zazikulu poŵelenga . Kodi Mau a Mulungu anaonetsa bwanji mphamvu yake m’zaka 100 zoyambilila ? * — Danieli 7 : 10 ; Chivumbulutso 5 : 11 . Yefita anasunga lonjezo limene anauza Yehova pamene anali kupita kukacita nkhondo ndi Aamoni , amene anali kuwopseza anthu a Mulungu . ( Ower . “ Zinthu zonse zimene zinalembedwa kalekale zinalembedwa kuti zitilangize , zimatipatsa ciyembekezo cifukwa Malembawa amatithandiza kupilila ndiponso amatilimbikitsa . ” — Aroma 15 : 4 . Woyang’anila sitediyamu , anakondwela ngako cakuti anatilola kucitilamo msonkhano popanda malipilo . Kodi Mumasankha Bwanji Zocita ? Inasintha zinthu padzikoli ndipo zimenezi zimatikhudza ngakhale masiku ano . ZIMENE ZINAYAMBITSA NKHONDO Pa Misonkhano ya Lateran ya m’caka ca 1123 ndi 1139 imene inali kucitikila ku Roma , anakhwimitsa lamulo lakuti azibusa sayenela kukwatila . Mwacitsanzo , pamene tipemphela monga banja tisanayambe kudya , anali kupinda tumanja twake , kuŵelama , na kuyankha na mtima wonse kuti “ Ame ! ” Ine pamodzi ndi mkazi wanga , Susan , ndi ana athu , Paul ndi Jesse Limbikitsani ena ‘ kugwila nchito ya mlaliki ’ Nimamvelako bwino nikapemphela kwa Mulungu . ” — Mateyu 26 : 39 . Ngati munthu umam’kondadi , umam’khulupililanso . Kodi mneneli wa ku Yuda amene sanam’tomole dzina , analephela kucita ciani ? Mwacidule , chulani mbali za cikondi zochulidwa pa 1 Akorinto 13 : 4 - 8 . ( Yak . 4 : 7 ) M’nkhani yotsatila tidzakambilana makhalidwe atatu amene tifunika kupewa kuti tipambane polimbana ndi Satana . Cofunika kwambili kuposa zonse n’cakuti Yehova amatisamalila mwauzimu . Amatipatsa ‘ mtendele wake umene umaposa kuganiza mozama kulikonse . ’ ( Afil . Mtsikana ndi m’busa wacinyamata anauzana zinthu zambili posonyezana cikondi . Kutumikila ku Taiwan kwandipatsa mwai wolaŵa cimwemwe cacikulu cimeneci . ” Cikhulupililo ca Mose mwa “ Wosaonekayo , ” cinam’thandiza pamene Aisiraeli anali pa mavuto aakulu atacoka mu Iguputo . Malinga ndi Salimo 41 : 4 , n’ciani cimene Davide anapempha kwa Yehova pamene anadwala kwambili ? ( Afil . 2 : 5 - 8 ) Ngati titengela cikondi cake cololela kuvutikila ena , mtima ndi maganizo athu zidzakhala ngati za Khristu , ndipo tidzayamba kuika zofuna za ena patsogolo osati zofuna zathu . Coyamba tili ndi Nsanja ya Mlonda imene imalembedwa m’cingelezi cosavuta . Tinapemphela kwa Yehova mocokela pansi pa mtima kuti atithandize ndi kutiteteza panthawi yovutayi . N’ciani cimadziŵikitsa gulu la Mulungu ? Kucokela nthawi imeneyo , sin’nachovenso njuga . Ndiye cifukwa cake Paulo ananena fanizo lina pambuyo ponena fanizo la kukhala ndi “ maziko olimba a Mulungu . ” Malo amene n’nali kugwilila nchito , anali odzaza ndi mapikica a zamalisece , kuphatikizapo a pa kompyuta . N’cifukwa cakuti anali kufunitsitsa kuteteza ubwenzi wake ndi Mulungu . Nditaceuka , ndinaona kuti wagwila kumutu uku akulila . ‘ Kukonda Mulungu ’ kumatilimbikitsa kukonda anzathu , maka - maka panthawi ya mavuto . Koma munthu wanzelu amakwanitsa kuseŵenzetsa cidziŵitso ndi kumvetsa zinthu panthawi imodzi kuti apindule . Ine na mkazi wanga wokondedwa , Elke Iwo anaona mmene Yehova anawatetezela pa ulendo wautali wobwelela ku dziko lawo . Kwa Akhristu a ku Kolose , kodi Paulo anapeleka malangizo ati a m’Malemba othandiza mabanja ? Baibo imachula za mkazi wina dzina lake Anna amene sanasiye kutamanda Yehova mu ukalamba wake . ( 1 ) Tiyenela kuyesetsa kukhazikitsa mtendele ndi m’bale wathu popanda kuloŵetsamo ena . ( b ) Kodi munthu ayenela kutsimikiza za ciani asanabatizidwe ? Baibulo limakamba mosapita m’mbali kuti ao amene satsatila malangizo a Mulungu ayenela kucotsedwa mumpingo . Kodi Goliyati anaganiza ciani ataona Davide ? “ Imfa , . . . monga mdani womalizila , idzaonongedwa . ” — 1 AKOR . Ambili analeka kutipatsa moni , ndipo anali kutiona ngati ocotsedwa . ” Kodi Mdyelekezi Ndani ? ( Deuteronomy 24 : 1 ) M’nthawi ya Yesu , panali masukulu aŵili a Arabi amene anali kuphunzitsa zinthu zosiyana ndi lamulo limeneli . Baibo imeneyo anaipulintila ku Nuremberg mu 1599 , ndipo anthu ambili amaicha Nuremberg Polyglot . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Tikufuna kucita zinthu zonse moona mtima . ” — Aheberi 13 : 18 . Kulimbana ndi makhalidwe oipa amenewa kumafuna kulimbikila . Koma n’zotheka kupambana pankhondoyi . Ndipo mosiyana ndi Rehobowamu , tidzaimabe nji pa kulambila koona . — Yuda 20 , 21 . Davide , amene anali m’busa komanso mfumu , anali ndi mabwenzi abwino . Ndipo pamene tiyandikila mapeto , m’pamene cidzakhala covuta kwambili kukhala maso . “ Malingalilo osautsa atandiculukila mumtima mwanga , mau anu [ Yehova ] otonthoza anayamba kusangalatsa moyo wanga . ” — Sal . Ngati aliko , anacokela kuti ? TSAMBA 10 • NYIMBO : 99 , 108 ( Gen . 37 : 23 - 28 ; 42 : 21 ) Pamene Yosefe anali ku Iguputo , anamunamizila kuti anafuna kugwilila mkazi wa mbuye wake , ndipo anaikidwa m’ndende popanda kuzengedwa mlandu . ( Gen . Utumikiwu ndi “ makalata oticitila umboni ” ndipo ndi wabwino kuposa kuchuka m’dzikoli . Kodi ali ndi dzina ? Tiyeni tikambilane mbali zitatu pamene tifunika kugwilitsila nchito cikumbumtima cabwino . Mbali zimenezi ndi ( 1 ) cithandizo ca mankhwala , ( 2 ) zosangulutsa , ndi ( 3 ) nchito yathu yolalikila . Monga mmene madzi amathandizila mbeu kukula bwino , kuyamikila wophunzila mocokela pansi pa mtima kudzamuthandiza kukula mwakuuzimu . — Yelekezelani ndi Mateyu 3 : 17 . Ngakhale ngati Akhristu anzake amukhumudwitsa , Mkristu wofikapo amayesetsa kulimbikitsa mgwilizano mumpingo . Ndiyeno bwanji akaona kuti iye akulankhulila atate ao . Paulo analemba kuti ngati Kristu sanaukitsidwe , ndiye kuti cikhulupililo ca Akristu ndi zimene amalalikila n’zopanda phindu . ( a ) Kodi Akhiristu analoŵa liti mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu ? Mwa ici , anthu ambili akhoza kuŵelenga Baibo imeneyi . Kumasulila mabuku onse a Malemba a Ciheberi kupita m’Cigiriki kunatha m’zaka za m’ma 100 B.C.E . ( 1 Akorinto 2 : 9 - 12 ) Ndipo coonadi cimene Yesu anakamba ndi ziphunzitso zolondola za m’Baibulo . Yesu Kristu ananena momveka bwino kuti : “ Pakuti moyo wosatha adzaupeza akamaphunzila ndi kudziŵa za inu , Mulungu yekhayo amene ali woona , ndi za Yesu Kristu , amene inu munamutuma . ” Apa Paulo anali kutanthauza kuti abale ake odzozedwa a m’nthawi ya atumwi akanapindula ndi nkhani zimene zinalembedwa m’Malemba . ( Akolose 3 : 14 ) Kukamba zoona , malinga n’zimene webusaiti ya Mayo Clinic inakamba , kukhululuka . . . Nanga kuli bwanji ise amene Mkulu wa Ansembe wathu ni Yesu ? Sitiyenela kukayikila ngakhale pang’ono kuti Mulungu ‘ adzaticitila cifundo ndi kutisonyeza kukoma mtima kwakukulu pa nthawi imene tikufunika thandizo . ’ — Aheb . ( 1 Tim . 2 : 3 , 4 ) Popeza “ palibe colengedwa cimene [ Yehova ] sangathe kuciona , ” ndife otsimikiza mtima kuti adzakokela ku gulu lake anthu amene “ amazindikila zosoŵa zao zauzimu , ” ndi kuwapatsa cakudya ca kuuzimu . — Aheb . Pitilizani Kusinkhasinkha Zinthu za Kuuzimu Ndi nthawi iti pamene tiyenela kukhala cete ? Akanafuna , iye akanakhala wacuma ndi wochuka popeza anali mtsogoleli wacipembedzo caciyuda . Koma anasiya nchito yake imeneyo kuti aike maganizo ake pa “ zinthu zofunika kwambili . ” Tiyeni tikambilane zinthu zinai zimene tingacite kuti tikonzekele . Munthu wodzicepetsa amazindikila kuti afunika kumakambitsana nthawi zonse ndi Atate wake wacikondi ndi wamphamvu zonse . Mofanana ndi anthu ambili , munthu wokaona malo ameneyu anacita cidwi kuona kuti Baibulo limakamba zoona zokha - zokha . Ŵelengani nkhani yotsatila , ndipo mwina mudzadabwa ndi yankho lake . Njila imodzi imene timapelekela zinthu “ za Mulungu kwa Mulungu ” ndi mwa kusatengako mbali m’mikangano ya ndale za dziko . Kutatsala tsiku limodzi kuti zimenezi zicitike , Mose analosela molunjika kuti : “ Maŵa m’maŵa , Yehova aonetsa amene ali wake . ” ( Num . Conco , sitiyenela kuyesa kugwilizanitsa mbali zonse - zonse za ukapolo wa Ayuda ndi zimene zinacitika kwa Akhiristu odzozedwa m’zaka zokafikitsa ku 1919 . Iwo anandiŵelengela 1 Akorinto 6 : 9 - 11 m’Baibulo . ( Mat . 19 : 25 , 26 ) Koma kuti tidzakhalebe ndi moyo ngakhale pambuyo pa ulamulilo wa zaka 1000 wa Yesu , tiyenela kucitapo kanthu tsopano kuti ‘ tigwile mwamphamvu ’ moyo wosatha . Cifukwa cakuti n’nali kusangalala nikamavutitsa ena , n’naphunzila mitundu yosiyana - siyana ya ndewo . Kucita izi kuyenela kuti kunali kum’thandiza kuonabe zinthu moyenela ndiponso kunam’tonthoza . — Sal . Kodi ofesi ya nthambi inamuuza ciani ? Katswili wa cikhalidwe dzina lake Antonio Cova Maduro analemba za Mboni za Yehova kuti “ pogwila nchito yolalikila zimakumana ndi mavuto ndipo zimalema kwambili . Koma zimapitiliza kugwila nchitoyi kuti uthenga wopatulika ufalikile padziko lonse lapansi . ” — El Universal Nyuzipepala ya Venezuela Timakondwela kwambili tikaganizila maulendo athu ocezela nthambi zosiyana - siyana . “ Tikudziŵa bwino ziwembu [ za Satana ] . ” — 2 AKOR . 2 : 11 . Mfundo zothandiza pophunzila buku lakuti “ Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni ” ni cida camphamvu cimene cingathandize acicepele na acikulile . Nanga muyenela kumva bwanji mukaona kuti ciŵelengelo ca amene amadya pa Cikumbutso cikukwela ? Iye anadalitsidwa cifukwa cokhala wokhulupilika kwa Yehova . Komabe coyamikilika n’cakuti , Akhiristu ambili amapeza njila zothetsela mavuto amenewa mwamtendele cifukwa coyang’ana kwa Mulungu . Anthu onse padziko lapansi adzakhala ndi nyumba zaozao , adzasangalala kugwila nchito yokhutilitsa , ndipo adzakhala ndi cakudya coculuka . — Ŵelengani Yesaya 9 : 6 , 7 ; 65 : 21 - 23 . 3 - 5 . ( a ) Ndi masautso otani amene Paulo anakumana nao ku Lusitara ? Cosankha ciliconse cinabweletsa mwayi kwa inu komanso maudindo . Madziwo anali ozizila ngako . Mtumwi Paulo anafotokoza kuti Yehova * “ ndi Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , amenenso amatitonthoza m’masautso athu onse . ” Aliyense akapatsidwa mbali , angapange kulambila kwa pabanja kukhala kwake - kwake . Pokhala otsatila a Yesu , ifenso tiyenela kukhala ndi mzimu wodzimana . Koposa zonse , mudzakhala pa ubwenzi wabwino na Yehova ndipo mudzapeza mtendele woculuka komanso wosatha m’dziko latsopano la Mulungu . — 2 Pet . Coyamba , onani zimene Mika 6 : 9 ikamba . Ndipo timakhala “ oona mtima ” mwa kupewa kutenga mbali m’ndale panthawi yovuta . Iwo anali kufunitsitsa kuniletsa kulalikila . Isimaeli , mwana wa zaka 19 wa Hagara , anapitiliza kuvutitsa Isaki wacicepele . TSAMBA 13 • NYIMBO : 98 , 102 Yohane 11 : 41 ) Ndipo pamene anali kufa , anapemphela kuti : “ Atate ndikuikiza mzimu wanga m’manja mwanu . ” Kuceleza munthu kungacepetse vuto la kukwesana ndi kuthetsa maganizo oipa amene mungakhale nawo okhudza munthuyo . Iwo amanena kuti Satana ndi ziwanda ndi anthu ongopeka amene amapezeka m’mabuku a nthano , m’mafilimu oopsa ndi m’masewela a pa kompyuta . Gulu la Yehova latulutsa Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lathunthu kapena mbali yake m’zinenelo zoposa 120 . Ndipo caka ciliconse amalitulutsanso m’zinenelo zina . ( 1 Akor . 15 : 48 , 49 ) Yesu sanapite kumwamba ndi thupi la nyama , naonso odzozedwa sadzapita kumwamba ndi matupi ao a nyama . Ndimawamvetsela akamakamba n’colinga cakuti ndidziŵe maganizo ao ndi zinthu zimene amakonda . Nthawi imene anafika pa nyumba , mtima wanga unali utatukutila ndi mkwiyo , ” anatelo a GEORGE . Panabwela dokota wina amene anali woledzela . Iye anayamba kunyoza atate cifukwa cosatengako mbali m’nkhondo . Cigawo ca mpukutu wa Yesaya cimene cinalembedwa zaka 100 Yesu asanabadwe , cinapezeka m’phanga pafupi ndi Nyanja Yakufa . 1 : 14 - 16 ) Khalidwe loyela limapangitsa kuti dzina la Mulungu lilemekezedwe . Conco , kudziŵa zimenezi kungatithandize kupilila mayeselo alionse ndi kusaopa imfa . N’zoona kuti Yesu anali atawatsimikizila kuti posacedwa adzalandila mzimu woyela . Pambuyo pake , mtumwi Yohane anakhala na mwayi wolalikila kwa Asamariya , ndipo utumikiwo unayenda bwino . Komabe , n’ciani cinacitika kuti mapangano akhale ofunika ? Cotelo lambilani Iye amene anapanga kumwamba , dziko lapansi , nyanja , ndi akasupe amadzi . ’ ” Kodi n’nadziŵa bwanji yankho ? Usakabwelenso kwa ine ! ” Pamene tiseŵenzetsa mfundo zimene taphunzila m’Baibo , timakhala na mtendele woculuka mu umoyo wathu . — Miy . Kukhulupilika kwake kunacititsa kuti akhale na mwayi wolalikila mwamuna wake ndi anthu ena . Mau amene analembedwa pa cipupa ca nyumba ina , akuonetsa kuti munthu wina dzina lake Theodotus , amene anali wansembe ndiponso mtsogoleli wa sunagoge , ndi amene “ anamanga sunagoge woŵelengelamo Tora . . . komanso nyumba yogona anthu ambili , zipinda , ndiponso mabeseni osungilamo madzi . ” Kodi cinthu cina cimene Yefita ndi Hana anali kufanana n’citi ? Afarao a ku Iguputo , mafumu , ndi ofufuza malo , onsewa anali kufuna kugonjetsa imfa . N’cifukwa Ciani Zinthu Zoipa Zimacitikila Anthu Abwino ? Ndipo zinaoneka kukhala zogwilizana na lemba la Aheberi 12 : 16 . ▪ Tikhale Ogwilizana Pamene Mapeto a Dzikoli Ayandikila “ Kodi Ndiyenera Kubatizidwa ? ” — mutu 37 Isaki atatsala pang’ono kubadwa , zofanana ndi zimenezi zinacitikanso ku Gerari . ( Gen . Chulani cinthu cimodzi cimene cingatilimbikitse . M’malo mwake anaunonga . Ena anali ‘ kunyenga anthu oona mtima . ’ Maina amene Satana anapatsidwa amaonetsa kuti iye ndi woipa kwambili . Ena amacita izi pa nthawi yopumula masana . M’bale wina wacinyamata dzina lake Patrick anacita zofanana ndi zimenezi . Nkhani ino ndiponso yotsatila zalembedwela makamaka akulu . Koma nkhanizi zikhudza onse mumpingo . Kukumbukila imfa ya Yesu caka ciliconse mwa njila imeneyi kumatipatsa mwai woyamikila cikondi cacikulu cimene Yehova ndi Yesu anationetsa . — Ŵelengani Luka 22 : 19 , 20 ; 1 Yohane 4 : 9 , 10 . Ndiyembekezela kuti mwina atate , amai , ndi acibale ena okondedwa adzalambila Yehova m’Paladaiso . Luigi anapemphela kwa Yehova kuti amuthandize kukhala wodekha . ( 1 Yohane 1 : 8 ) Mukacita zimenezi , ana anu acinyamata adzaphunzila kuti ayenela kuvomeleza akalakwitsa , ndipo adzakulemekezani kwambili . Koma dzina langa ndine Inoki . TSIKU lina , munthu wina amene anali ndi munda wa mpesa anacelela ku msika kukasakila anthu aganyu . Ŵelengani Yesaya 40 : 29 . Ngakhale kuti kucita zimenezi sikunali kopepuka , Yehova anandithandiza kuti ndikwanitse kucokamo . Pambuyo pake , n’nayamba kupepanso camba . Motelo anasandutsa madzi okwana malita 380 kukhala “ vinyo wabwino . ” Ngati ndinu wacicepele wobatizika kapena amene mufuna kudzabatizika , kodi mungalimbitse bwanji ubwenzi wanu na Yehova ? Tikakhala na nkhawa , Yehova ni wokonzeka kutitonthoza ndi kutitsitsimula . ( Sal . Ulaliki wathu ungakhale wotsitsimula tikamagwilitsila nchito njila zosiyanasiyana pophunzitsa anthu coonadi . Conco , anatenga kansalu n’kumanga cala cimene anadzicekaco , ndipo anayenda wapansi kukapeleka kalatayo . M’matauni atatu cabe a m’delali , muli mipingo 50 na ofalitsa oposa 5,400 . Seŵelo la “ Eureka X ” linali ndi mau onse a wosimba ndi tunyimbo twabwino . Koma pakubuka mafunso ena . Timapeza thandizo pa nthawi yoyenela . Alongo aŵiliwa anabwelela ku famu pambuyo pa masiku atatu , koma bwana wao sanadziŵe kuti anali atacokapo . Atate akacokapo , amayi anali kuuza ine ndi mlongosi wanga zimene aphunzila . Nili mnyamata , n’naphunzila kuyendetsa thilakita na nchito zina zaulimi . Munthuyo mukamupeza , nonse aŵili muyenela kucita khama kuti cikondi canu cilimbe . ( 1 Mafumu caputala 18 ) Onani nkhani za mutu wakuti “ Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo ” zopezeka m’magazini a Nsanja ya Olonda a January 1 ndi April 1 , 2008 . Ena mwa mavutowa ndi kucita cigololo , kugonana kwa amuna kapena akazi okhaokha , kapena kugonana ndi wacibale . Ndipo ana sangazicita bwino ku sukulu , angakhale aukali , ankhawa , ovutika maganizo kapena angakhale ndi maganizo ofuna kudzipha . [ Cithunzi papeji 19 ] ( Agalatiya 6 : 1 ) Koma tonse tikhoza kuthandizako abale ndi alongo acikulile , kapena mabanja ena amene akukumana ndi mavuto . N’cifukwa cake anadzipeleka kuti akamenyane na Goliyati . — 1 Samueli 17 : 32 . Koposa zonse , kumbukilani kuti Mulungu wakupatsani udindo waukulu wolengeza uthenga wabwino monga Mboni yake . ( Yes . ‘ Fikani . . . pa msinkhu waucikulile umene Kristu anafikapo . ’ — AEFESO 4 : 13 . Yesaya 40 : 26 Nthawi zonse pamene nicita izi , m’pamenenso amanidalila kwambili . ” — Sarah . M’malomwake , amayembekezela moleza mtima “ zipatso zofunika kwambili zotuluka m’nthaka . ” Kupatsa na kuthandiza ena kumabweletsa cimwemwe cacikulu , maka - maka ngati tiwathandizanso kudziŵa bwino Gwelo la mphatso zonse zabwino — Yehova Mulungu . “ Mulungu Akhale Woona . ” Iwo anali kutumikila mu mpingo wa citundu ca manja ku Japan . Koma anali kudziŵa kuti panali nchito yaikulu imene inali kufunika kucitidwa , ndi kuti anthu ambili adzalandila uthenga wabwino . Caka ciliconse , tinali kukonza ndi kusunga zipatso ndi ndiwo zamasamba zodzaza zitini 45,000 monga cakudya ca banja la Beteli . 14 Kuteteza Uthenga Wabwino Pamaso pa Akulu - akulu a Boma Tikakhala ndi cikhulupililo colimba mwa Mulungu , tifunika kupitiliza kucionjezela . Koposa zonse , mukamaima pang’ono ndi kusinkhasinkha pa zimene mwaŵelenga , cofalitsaco cidzakukhuzani mtima . 6 : 33 ; Maliko 13 : 10 . Patapita nthawi , tinakukila ku Hollywood , mu mzinda wa Florida , kufupi na acibululu a amuna anga . Kwa zaka zambili , banjali linathandiza anthu ambili ocokela kumaiko ena kukhala atumiki a Yehova . N’cimodzi - modzinso na ophunzila Baibo masiku ano , kaya ni acicepele kapena acikulile . Pitilizani kulimbitsa cikhulupililo canu mwa kuŵelenga Baibo , kukonzekela misonkhano na kupezekapo , kulalikila , ndi kupemphela kwa Mulungu kuti akupatseni mphamvu zokuthandizani kupilila . Iye anaseŵenzetsa nthawi yake yopumula pocita zinthu zolimbitsa ubwenzi wake na Yehova . Zimene mwininyumba angayankhe zidzakuthandizani kudziŵa zimene mungaŵelenge ndi kukambilana m’kapepalako . ( a ) Ndi malemba ati amene aonetsa kuti Yehova adzaononga imfa ya Adamu ? Tinali ana 12 ndipo atate anali ndi nchito yotidyetsa , pamene amai sanali kufuna ngakhale pang’ono kuti anafe tizilova ku chalichi . Iye amadziŵa zimenezi , ndipo cifukwa ca cikondi cake anatipatsa dipo kudzela mwa Khristu . Iye anadalitsa kwambili Aisiraeli amene anali ndi mtima wofunitsitsa kupeleka mwa kuwatsogolela , ndipo anthuwo anali kukhala acimwemwe . N’zoona kuti kulalikila ndi kuphunzitsa n’kofunika , koma zimenezi sizingapose pa kukhala wopanda cifukwa cotinenezela , wosacita zinthu mopitilila malile , woganiza bwino , wadongosolo , woceleza alendo , ndi wololela . ” Ofalitsa atsopano amene akalibe kubatizika ayenela kudziŵa cifukwa cake kucita phunzilo laumwini n’kofunika . 12 : 10 - 13 ) Kucita zimenezo kudzakuthandizani kulimbitsa cikhulupililo canu ndi kupewa kupanga zosankha zoipa cifukwa cosonkhezeledwa ndi anzanu , kutengela maganizo a dziko , kapena cifukwa cofuna kudzisangalatsa . Phunzitsani acatsopano kuti azikonda Akhiristu anzawo ( Onani ndime 13 , 14 ) A Zimba : Ndiganiza kuti ndi Mulungu . Palinso vuto lina limene anthu ena a pabanja amakumana nalo . Jacob ndi makolo ake amakonda kuceza ndi abale a pa Beteli a mumpingo Kodi kuukitsidwa kwa Lazalo kumaonetsa kuti Yesu ndi munthu wotani ? Tengelani Citsanzo ca Atumiki Okhulupilika a Yehova , Feb . Kwa zaka zambili , anthu akhala akucita cidwi na nkhani ya paradaiso . Nyimbo za m’buku lakuti ‘ Imbani Mokweza ndi Mosangalala ’ kwa Yehova , ’ zinaikiwa mogwilizana na nkhani zake kuti tisamavutike kuliseŵenzetsa . Ngati ayi , zidzakhala ngati ‘ mukungomenya mphepo , ’ ndipo mungalephele kugonjetsa adani anu . Kingsley ndi wakhungu ndipo amakhala ku Sri Lanka . Pamene Yesu anakamba kuti kapolo mmodzi pa akapolo atatu aja anali woipa ndi waulesi , iye sanali kutanthauza kuti odzozedwa ena adzakhala monga kapolo ameneyo . Pafupi - fupi pa nyumba iliyonse tinali kupeza anthu omvetsela , ndipo tinali kuwatambitsa mavidiyo yathu , ndi kuwagaŵila zofalitsa . ” Iwo kawili - kawili amaonetsedwa kuti akutumikila pamaso pa Mulungu . — Genesis 3 : 24 ; Ezekieli 9 : 3 ; 11 : 22 . Kudziŵa mbali zimenezi kungalimbitse cikhulupililo cathu . Conco , tiyeni tione zimene Malemba amakamba pa mafunso amenewa . Masiku ano , abale amene ali ndi ana aang’ono panyumba saikidwa kukhala woyang’anila dela . Abale ndi alongo a ku Poland m’dziko la France akupita ku msonkhano . Thanzi yangwilo ndiye tsogolo la anthu okhala padziko lapansi . Akatsiliza kuukanda anali kuyamba kuphika mkate . ( Mat . 13 : 16 ) N’cifukwa ciani ophunzila a Yesu anali kumvetsetsa zimene iye anali kuphunzitsa pamene ena anali kulephela ? Iye angayamikile kwambili ngati mum’thandiza kutsatila bwino pulogilamu na kupeza malemba amene akuŵelengedwa . Iye “ sanganame . ” Koma tifunse motele : Kodi mudzaonetsa kuti mumayamikila zimene munalandila ? Kodi mtumwi Paulo anaonetsa bwanji kuti kulimbikitsa ena n’kofunika ? Pakabuka mikangano , maboma ena amalimbikitsa nzika zao kutenga mbali m’ndale . N’tatsiliza maphunzilo a miyezi iŵili a Sukulu Yophunzitsa Baibo ya Abale Osakwatila , * ananitumiza ku gawo lina kumene n’nayamba kutsogoza maphunzilo anayi a Baibo . ( Onani mau amunsi . ) ( b ) Kodi tingalimbitse bwanji ubwenzi wathu ndi Yehova ? Posakhalitsa , iwo anayamba kusintha zina na zina kuti akwanilitse colinga cawo . ( b ) Kodi “ ana aakazi a mafumu ” ndi “ mkazi wamkulu wa mfumu ” amene akusangalala pamodzi ndi Mkwati ndani ? NYIMBO : 91 , 13 Meya wa mumzindawo anabwela . “ YEHOVA NDI MTENDELE ” 7 - 9 . ( a ) Kodi ndi zinthu zocititsa cidwi ziti zimene zinacitikila Gidiyoni ? Iye anawalamula kuti : “ Pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzila anga . ” Zakugwa mwadzidzidzi monga ngozi kapena matenda , zimatipatsa mwai woonetsa cikondi ceniceni cacikristu . ( Agal . 6 : 2 , 5 ; 1 Pet . Pokhala Mboni za Yehova zodzipeleka , timakhulupilila kuti tili ndi coonadi , ndipo timazindikila udindo wathu wophunzitsa ena uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . 46 : 10 ; 55 : 11 ) Munthu akadziŵa mfundo zopezeka m’Mau a Yehova , zimene amaŵelenga m’Baibulo zimakhudza kwambili umoyo wake . Cotelo , zinthu zinasinthanso pakati pa anthu a Mulungu . Timalimbikitsanso mtendele mwa kukamba mwaulemu kwa akulu - akulu a boma , olo amene amatsutsa nchito yathu . 7 : 9 . 14 : 22 . Kodi inuyo mudzacita ciani ? Zimenezi zidzakuthandizani kukonzekela ubatizo . Ine ndipitiliza kukugaŵilani cakudya limodzi ndi ana anu . ” — Genesis 50 : 21 . N’tatsiliza maphunzilo , n’nabwelela ku Pakistan , kumene nthawi zina n’nali kutumikila monga woyang’anila dela . Ni mavuto ati amene anthu amakumana nawo kunchito masiku ano ? Titafika mu mzindawu , panali cabe kagulu kamodzi kutali ndi tauni . Panalinso nyumba ya amishonali mmene munali kukhala alongo anayi : Esther Tracy , Ramona Bauer , Luiza Schwarz , ndi Lorraine Brookes ( tsopano amachedwa Lorraine Wallen ) . Nkhaniyi , ifotokoza mmene Mulungu anali kupatsila anthu ake malangizo ndi malamulo atsopano nthawi zonse zinthu zikasintha . Inali sukulu ya mwezi wathunthu ya akulu , oyang’anila madela , na oyang’anila zigawo . ( a ) Ndi zinthu zotani zimene tingasinkhesinkhe ? Nzelu zopindulitsa zimasiyana ndi cidziŵitso komanso kumvetsa zinthu . Sikuti anadzidalila kwambili ayi , komanso sanakhwethemuke cifukwa ca mantha . Ndipo ofesi ya nthambi imatithandiza kugwilitsila nchito malangizo ocokela kwa kapolo wokhulupilika . Muyenela kukhulupilila kuti Mulungu , amene anatipatsa moyo , ali na mphamvu zoukitsa akufa . Onani zimene Baibo imakamba zokhudza maulosi monga amenewa : Yehova Mulungu , amene ndi Mlengi , sanalenge anthu n’colinga cakuti akhale ndi moyo kwa zaka zocepa cabe kenako n’kufa . Mphatso imeneyi inapelekedwa n’colinga cakuti ‘ tidzapeze moyo . ’ ( 1 Yoh . Zimenezi zinacitikilanso tate wina dzina lake Ronald . Kwa zaka zambili , Mariya ayenela kuti anali kusinkhasinkha maulosi onena za mwana wake . Iye anali kudziŵa kuti Yesu adzachedwa “ Mwana wa Wam’mwambamwamba . ” Mwacitsanzo , ine na amuna anga tinali na mwayi woonelela maubatizo a ophunzila Baibo athu okwana 136 . Mwacitsanzo , ngati m’Nyumba ya Ufumu muli cipinda cina mmene angathe kumvetsela misonkhano , io angakhale mmenemo . Kuwonjezela apo , ofesi ya nthambi inali itasankha kuti m’dzikolo mukhale cabe apainiya pafupi - fupi 200 , amene anali kutumikila m’magawo akutali osati m’mipingo . Conco , kulandila Baibulo ndi mwai wamtengo wapatali . 24 : 67 ) Masiku ano , timayamikila kwambili kukhala ndi akazi oopa Mulungu pakati pathu , amene ali ngati Sara ndi Rabeka ! Mbili imaonetsa kuti izo sizinatengeko mbali m’nkhondo . N’cifukwa ciani anasankha kusindikiza buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu ? 3 : 36 ) Ndife okondwa kuti nsembe ya Khiristu imacititsa kuti zikhale zotheka kukhala mabwenzi a Mulungu . Mwina munganize kuti kukambapo pa colakwaco kudzawononga ubwenzi wanu . ( Aroma 5 : 10 ) Kuyanjanitsidwa kumeneko kunatithandiza kuti tikhale pamtendele ndi Yehova . Yesu anakamba kuti : “ Odala ndi amene akumva mau a Mulungu ndi kuwasunga . ” Taphunzilanso ubwino wokulitsa mikhalidwe ya cipatso ca mzimu wa Mulungu , kuuzako wina nkhawa zanu , na kupeza cilimbitso cauzimu ku mpingo . Koma titafika kumeneko , woyang’anilayo anatiuza kuti : “ Timakudziŵani , ndipo timalemekeza cosankha canu . ( 1 Akor . 9 : 19 , 23 ) Ena a iwo amatumikila m’magawo awo , ena anakukila kosoŵa . Cofunika n’ciani kuti ciyamikilo cathu cikhale cogwila mtima ? Tikatelo , cidzakhala copepuka kudziŵa zimene Yehova afuna kuti ticite . N’cimodzimodzi ndi Yosefe . Iye anali “ mwana ” wa Heli , popeza kuti anakwatila Mariya , mwana wa Heli . Titatenga maviza athu , tinayamba kucita lendi nyumba ina . Kodi Paulo anawaona bwanji aja amene analikutumikila Yehova mwakhama ? Nthawi zina , sitingaone dzanja la Mulungu pa umoyo wathu . 5 : 14 ) N’ciani cimene tingakambe polimbikitsa anthu aconco ? Kulimba mtima komanso cikhulupililo ca asilikaliwo cinali kudzayesedwa patsikuli ngakhale kuti anali 10,000 cabe . Pofika m’cilimwe ca mu 1914 , anthu mamiliyoni a m’mizinda ikuluikulu anasonkhana kuti apenyelele “ Seŵelo la Cilengedwe . ” Filimu ya maola 8 imeneyi yofotokoza zinthu zakale , inakonzedwa ndi Ophunzila Baibulo . Zinthu zina zonse zinalengedwa kudzela mwa iye , ndiponso cifukwa ca iye . ” Akristu oona anacita khama kuthetsa cinyengo ciliconse cimene anali naco . Mwacitsanzo , anthu ocokela kumayiko ena amakhumudwa na mavalidwe ena a azimayi kulingana ndi cikhalidwe cakwawo . Kodi n’zocitika ziti zimene zingacititse ana kupeleka thandizo lalikulu kwa makolo ao ? Iye anali wocokela mumtundu wa Arefai , anthu amene anali kudziŵika kuti anali atali - atali kwambili . 20 “ Tipita Nanu Limodzi ” Gener anayamba kukhala ndi moyo waciphamaso . 8 : 3 , 4 ) Mwacitsanzo , milalang’amba ili ndi nyenyezi mamiliyoni ambili , koma zonsezo zimayenda mwadongosolo . Ndi Mboni za Yehova zokha . Kodi Tili mu “ Masiku Otsiliza ” ? Kuti Mulungu avumbulile anthu zimene zinali kudzacitika mtsogolo , anagwilitsila nchito angelo , masomphenya kapena maloto . Poyamba , anthu a Mulungu anali kugwilitsila nchito Baibulo la King James Version , limene anamaliza kulimasulila mu 1611 . Taganizani zimenezo ! Poyamba , atate ŵake ayenela kuti anali kulambila mafano . Kodi makolo ayenela kucita ciani kuti aŵete ana ao ? Ngakhale kuti mwamuna wake palibe , iye adziŵa mmene mwamuna wakeyo angamvelele ngati wagula nsapato zodula . Nanga mavuto akakukulilani msinkhu , kodi mumapeza kuti citonthozo , cilimbikitso , na malangizo odalilika ? Tsopano papita zaka kucoka pamene mwamuna wanga anandisiya , koma ndimasungulumwabe ndipo ndimadziona kuti ndine wacabecabe . N’zosangalatsa kuti cimodzi mwa zolinga za misonkhano n’cakuti ‘ tizilimbikitsana , ndipo tiwonjezele kucita zimenezi , makamaka pamene tikuona kuti tsikulo likuyandikila . ’ Mungapambane Polimbana Ndi Satana “ Seŵelo la Cilengedwe ” ndi “ Seŵelo la Eureka , ” linathandiza anthu kukhulupilila Baibulo kuti ndi lolondola kwambili pankhani ya sayansi , ndi kuti lili ndi malangizo othandiza kwambili pa umoyo . Koma Mau a Mulungu anakambilatu kuti maboma ndi mabungwe awo adzagwedezeka n’kucoka pa maziko awo . Kenako mukumva Yehova akukuuzani kuti : “ Mwana wanga , khala wanzelu ndi kukondweletsa mtima wanga , kuti ndimuyankhe amene akunditonza . ” — Miyambo 27 : 11 . Kupatukana kungabweletseko mpumulo winawake . ( a ) N’ciani cingatithandize kuti tikule mwauzimu ? Conco , amatipempha kuti tizicita zinthu zom’kondweletsa kuti tikalandile madalitso ake . ( Miy . 3 : 5 , 6 ) M’malomwake , mofanana ndi msilikali amene anali kuonetsetsa kuti tunsimbi twa codzitetezela pa cifuwa n’togwila bwino , tifunika kuonetsetsa kuti mfundo za Yehova ni zozikika mozama mu mtima mwathu . ▪ Muzimvetsela Mau a Yehova Kulikonse Kumene Mungakhale Panthawi ino , ‘ tidzakhalabe okhutila ndi zakudya ndi zovala ’ zimene tili nazo . Koma panthawiyi , anapeza ngale yamtengo wapatali kwambili cakuti atangoiwona , anakondwela ngako . Tatenai analamulila cigawoci kucokela ca m’ma 520 mpaka 502 B.C.E . Mu 1970 , ndinabwelela ku Hungary , ndipo kumeneko ndinakumana ndi Rose amene anadzakhala mkazi wanga . Yehova Adzakucilikizani Zinthu zambili zikucitika mumzindawo . Muyenela kudziŵa zimenezi cifukwa cakuti Mulungu wapeleka malonjezo ambili okhudza zamtsogolo amene adzakukhudzani . Mivi ina “ yoyaka moto ” imene Satana angakuponyeleni ndiyo kufalitsa mabodza akuti Yehova sakuonani monga ofunika ndiponso sakukondani . Koma mwadzidzidzi , iye anamva m’mala kuŵaŵa . Ndiye cifukwa cake banja liyenela kukonzekela pasadakhale . Pa Mateyu 6 : 34 ( ŵelengani ) , pali malangizo a Yesu othandiza akuti : “ Musamade nkhawa . ” ( b ) Ndi kukambitsilana kwina kuti kumene inu mwapeza kuti n’kothandiza ? Nafenso tikakumana na mavuto , tifunika kumuuza Yehova mmene timvelela . Koma tifunika kucita zambili kuposa pamenepa . Ine na Tony tinabatizika monga Mboni za Yehova mu July 1982 . m’banja ? Koma ena amene amasonkhanitsidwa amakhala monga nsomba “ zosafunika ” cifukwa sakhala ovomelezeka kwa Yehova . Payenela kukhala zifukwa zingapo . Mwacitsanzo , Dixon analosela kuti Nkhondo Yacitatu ya Dziko lonse idzayamba mu 1958 , ndipo Cayce analosela kuti mu 1975 mzinda wa New York udzamizidwa ndi madzi . Tiyeni tikhale m’gulu la anthu amene ‘ adzatamanda Mfumu mpaka kalekale , ndithu mpaka muyaya . ’ 26 Mbili Yanga — N’natonthozedwa pa Mavuto Anga Onse Maluwa amenewa satunga nsalu kapena zovala ndi kuzivalika kuti aoneke okongola . 17 , 18 . ( a ) Timagwilizana nalo bwanji Bungwe Lolamulila ? Ndipo abale amene anacoka ku Austria , poyamba anali kuyewa umoyo wa kwao . Mosakaikila alangizi anu akusukulu amadziŵa bwino nchito zimene zili m’dela lanu . Anthu okonda ndalama sangakondweletse Mulungu . Conco , simufunika kucita kudzipha kuti mpaka mugule ciwiya coloŵela pa jw.org . 13 : 5 . Koma Aisiraeli ena anakhala osakhulupilika . Ana a Aroni sanali kuimila nkhosa zina za Yesu kapena kuti a “ khamu lalikulu . ” ( Chiv . Mmene cilengedwe cilili ca dongosolo ni umboni wakuti Mulungu ali nalo colinga cabwino dziko lapansi ndi anthu . Ngati timamvetsetsa coonadi ca m’Baibo , zimakhala ngati kuti tacimanga kwambili m’ciuno mwathu . Ndipo zinthu zikalakwika , amakonda kuimba mlandu ena , m’malo movomeleza kulakwa kwawo . Makhalidwe oipa afala kwambili , ndipo izi zikuonetsatu kuti ino ndi “ nthawi . . . yovuta . ” Nthawi zonse muzidalila Yehova kuti akuthandizeni kupeza zosoŵa zanu za kuuzimu ndi zakuthupi . Ngati ‘ tiika maganizo pa zinthu za mzimu , ’ timakhala pamtendele na Mlengi wathu . Kapena kodi zikanakuvutani kulamulila mkwiyo wanu ? Pomaliza pake , Msulami anaitana wacikondi wake kuti abwele mothamanga kwa iye “ ngati insa . ” — Nyimbo 8 : 14 . Ukulilenji umboni woonetsa cikhulupililo na cikondi ceni - ceni ca Akhiristu ! Satiyelekezela ndi anthu ena , ndipo tikalakwitsa saleka kutikonda . 5 . Mau a Yohane oyamikila Gayo cifukwa coceleza abale , aonetsa kuti Akhristu ocokela m’mipingo yosiyana - siyana anali kupita kaŵili - kaŵili kumene kunali kukhala mtumwi Yohane . Mwacionekele , Akhristu amenewo anali kufotokozela Yohane mmene ayendela pa ulendo wawo . Mau amenewa anandikhumudwitsa kwambili . Ngati tacita zimenezo , Yehova sangakhale “ Yehova mmodzi ” kwa ife . Panthawiyo , “ Yehova anaona kuti kuipa kwa anthu kwaculuka padziko lapansi , ndipo malingalilo onse a m’mitima ya anthu anali oipa okhaokha nthawi zonse . ” Monga banja la Mulungu , io anafunikila kulambila Yehova kosatha pamodzi ndi angelo . Anakambanso kuti : “ Sikuti nthawi zonse amagwilizana ndi ziphunzitso zathu . Koma kuyambila nthawiyo , anaona kuti kugwilizana na Mboni za Yehova kunali kusintha umoyo wanga . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Kodi wamuona munthu waluso pa nchito yake ? Yosimbidwa ndi Ernest Loedi Ndikuthandiza ” ? N’cifukwa ciani ndise otsimikiza kuti zigamulo za Yehova n’zolungama ? Iye anadziŵa zimene womupelekayo anali kufuna kucita . Cifukwa cakuti kusintha kumeneku kunapangidwa potsatila zimene Malemba amasonyeza . ( Mat . 6 : 21 ) Kuti tidziŵe zimene zili mumtima mwathu , ndi bwino kudzifufuza nthawi zonse . Iye amaona mmene mtima wao ulili ndipo adziŵa kuti kupanda ungwilo kudzatha posacedwapa . Asanayankhe , amaiwo anayamba aganiza , kenako anakamba kuti : “ N’zoona kuti mwanayu sakundimvela , koma ndikali kumuphunzitsa . Colinga ca bungweli ndi “ kukhazikitsa mgwilizano wa zipembedzo wokhalitsa . ” Zimenezi zinandipatsa mwai wakuti ndikhale wakuba m’mabanki . Potsutsa ziphunzitso zabodza zacipembedzo , iye sanaseŵenzetse nzelu zake zakuya kapena cidziŵitso cake . Coonadi candithandiza kukhala wokhutila ndi wacimwemwe . ” N’ciani cinam’thandiza kukhalabe wokhulupilika kwa m’busayo panthawi imene anali kukhala motalikilana ? Ciyeso citatha , Yehova anapatsa Yobu zinthu zimene anali nazo poyamba , kuŵilikiza kaŵili . Komanso anamuonjezela zaka zina 140 . Tifunika Kukhala Bwanji Popemphela ? Izi si zimene Baibulo limaphunzitsa . Kodi kukhala wodzicepetsa kumabweletsa madalitso anji ? Mboni zina zinali kuicha kuti Aroni cifukwa galamafoni inali kulankhula m’malo mwa io . ( Mateyu 19 : 5 , 6 ) Pa lembali tipezapo mfundo ziŵili zofunika kwambili . M’kupita kwa nthawi , anthu ambili okhala na ciyembekezo ca padziko lapansi anayamba kugwilizana ndi odzozedwa . Anthu okhala na ciyembekezo ca padziko amenewa ndi amene akuimilidwa na ndodo “ ya Yosefe . ” Tisanakhale Mboni , tinafunika kuleka kucita zinthu zimene Yehova amadana nazo . 18 , 19 . ( a ) Kodi mapangano amene takambilana atsimikizila ciani ponena za Ufumu ? Timakulitsanso cimwemwe cathu mwa kuganizila madalitso amene tili nawo , kutengela cikhulupililo ca ena , na kuyesetsa kucita cifunilo ca Mulungu . Tikamacita zimenezi , mau a pa Salimo 64 : 10 adzakwanilitsika mu umoyo wathu . Kodi n’ciani cikanamutonthoza ? Zina mwa mbalame zimenezi zinali kumanga zisa m’kacisi amene Solomo anamanga . Padziko lonse lapansi , pafupifupi 30 pelesenti ya akazi amamenyedwa ndi amuna ao , kapena zisumbali zao . Kulekelela dzimbili pa citsulo kungacititse kuti cionongeke . 48 : 17 , 18 . Cilamulo cinathandiza Aisiraeli kukonzekela cocitika cofunika kwambili pokwanilitsa cifunilo ca Yehova . Cocitika cimeneco ndi kubwela kwa Yesu Kristu , yemwe ndi Mesiya . Zimene zinacitika mu mzinda wa Florida ku America , zionetsa kuti mfundo imeneyi niyoona . Mukatelo mudzathandiza wophunzila kukhala wofunitsitsa kutumikila Mulungu , ndipo mudzaonetsa kuti mumatsatila Yesu , Mphunzitsi Wamkulu . M’malomwake , anapatsa Yobu mpata woonetsa kukhulupilika kwake , kuti zidziŵike kuti sanali kulambila Mulungu cifukwa ca dyela koma cifukwa com’konda na mtima wonse . Mvelani zimene zinacitikila mpainiya wina amene tam’patsa dzina lakuti Lucy . Cifukwa ca dyela , Sauli anatenga zinthu zimene Mulungu analamula kuti zionongedwe . Palembali , Yesu anali kukamba zimene munthu afunika kucita ngati wina wamucitila colakwa cacikulu . Ena angakambe kuti : ‘ Mulungu ni wanzelu kwambili ndipo amadziŵa zonse cakuti akanakwanitsa kulemba Baibo m’njila yosavuta kumva kuti aliyense azitha kuimvetsetsa . Zinthu masiku ano n’zofanana ndi mmene zinalili m’nthawi ya Ezekieli . Panthawiyo , zocita za Ayuda zinakhudza mmene anthu a mitundu ina anali kuonela dzina la Yehova . — Ezek . Cizindikilo ca “ mapeto a nthawi ino ” cimene anakamba , ciphatikizapo zocitika monga nkhondo pakati pa mitundu , njala , milili , na zivomezi zamphamvu . Sitingaganize conco ngati timadziŵa bwino njila za Yehova . M’malomwake , anaika maganizo awo pa nchito imene Yesu anawapatsa . — Machitidwe 5 : 42 . Kodi n’cifukwa cakuti wapanikizika ndi sukulu , kapena akulimbana ndi matenda aakulu ? N’cifukwa ciani tinamasuliwa ku ukapolo wa ucimo na imfa ? ( Aefeso 5 : 1 , 2 ; 1 Petulo 2 : 21 ) Mwacitsanzo , mwina timakonda kudandaula kapena kunena anthu ena . Muyenela kufutukula mtima wanu . Nanga Akhristu ena acita zotani cifukwa ca maganizo olakwika ? Kodi n’koyenela m’bale kusunga ndevu ? Cifukwa cakuti Yesu anali wodzipeleka ndi mtima wonse , Yehova anamudalitsa pa utumiki wake padziko lapansi . Yesu atapeleka moyo wake monga nsembe ndi kuukitsidwa , Mulungu anam’patsa mphoto . M’zaka za m’ma 1500 , patapita zaka 300 kucokela pamene Langton anagaŵa Baibulo kukhala m’macaputala , katswili wina wodziŵa nchito yopulinta mabuku , Robert Estienne anapeputsanso zinthu pamene anagaŵa Baibulo kukhala m’mavesi . Nanga atithandiza bwanji kudziŵa zimene tingacite kuti tithaŵile kwa Yehova masiku ano ? Ngati mufuna kudziŵa zambili pa zimene iwo adzacita , kambani na Mboni za Yehova , kapena pitani pa webusaiti yathu ya www.jw.org , na kucita daunilodi buku la Zimene Baibo Ingatiphunzitse . Conco kupitila mwa mneneli Yeremiya , Mulungu anati : “ Taonani ! Ulosiwo ukunena zimene zidzacitika m’masiku otsiliza a dziko loipa lino Yesu akadzayamba kulamulila mu Ufumu wa Mulungu . Kodi ufulu wokhala ndi malile ni ufulu weni - weni ? Kodi anthu ocita zabwino ali na tsogolo yabwanji ? — Vesi 11 , na 29 . Akamaganizila za moyo wao akali ana , amawawidwa mtima cifukwa ca nkhanza imene atate ao anawacitila . M’nkhanizi zidzamvetsa tanthauzo la kudzicepetsa . Luka anali dokotala ndipo anali kuyendela pamodzi ndi Paulo . Ena anali kuseŵenzetsa tumizela twa pa tsamba la tiyi , kapena pa njele ya khofi . N’tatsala pang’ono kucoka , iwo anayamba kuimba nyimbo ya Ufumu . ZAKA zoposa 30 zapitazo , Osei wa ku Ghana amene sanali Mboni panthawiyo , anayenda ku Europe . ( Salimo 46 : 9 ) Tikukupemphani kuti muphunzile za Ufumu umenewo kuti mudzakhale ndi moyo pa nthawi imene mtendele udzadzaza dziko lonse lapansi . — Yesaya 9 : 6 , 7 . Tiyenelanso kusinkha - sinkha za citsanzo cabwino ca Mwana wake , Yesu Kristu , ndi kuyesetsa kumutsanzila . Imakamba Zoona pa Nkhani za Sayansi : Baibo si buku ya sayansi . Koma ikamakamba za sayansi , imakamba zoona ndipo mfundo zake zinali zotsogola kwambili asayansi asanazitulukile . M’malo mwake , dzifunseni kuti : ‘ N’cifukwa ciani nchito imeneyi ndi yofunika ? Tinali kumufotokozela kuti mbili yake siingawonongeke malinga ngati waongolela zimene walakwitsa , ndipo ise tilipo kuti tim’thandize kucita zimenezo . ” — Daniel . Ife anthu sitinalengedwe kuti tizikumana ndi imfa mu umoyo wathu . Charles , tate wa ana atatu a zaka za pakati pa 9 mpaka 13 , amasonkhana ku kagulu kokamba Cilingala . TSAMBA 7 • NYIMBO : 65 , 64 Kodi akazi anam’tumikila bwanji Yehova m’nthawi zakale ? M’bale Mumba : Ndakubweletselani Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani ! Tsopano tiyeni tikambilane makhalidwe ena a Yesu ocititsa cidwi . 7 - 9 . Kodi phunzilo laumwini limaphatikizapo ciani ? Pamisonkhano timaphunzila zambili . Popeza kuti tikukhala m’dziko lino , zilizonse zimene anthu angacite pofuna kuthetsa nkhani zimenezi zingakhudze ife kapena mabanja athu . Pankhondo yaciŵili ya padziko lonse , ndi pamene anthu anaphedwa kwambili . Ophunzila ake anaona kuti iye anadzipeleka kuti atumikile Yehova ndi anthu , ndipo naonso anaphunzila kucita cimodzimodzi . Zimene tingacite potamanda Yehova zimadalila mmene thanzi lathu lilili , koma tiyenela kupeleka nsembe zabwino koposa . — Aroma 12 : 1 ; 2 Tim . Mtumwi Paulo anauzilidwa kulemba kuti : “ Anthu adzakhala odzikonda . ” 106 : 7 , 11 - 13 . Mwaukali mkulu wa asilikaliyo anauza M’bale Rutherford kuti : “ Pulezidenti Wilson [ wa dziko la America ] ni amene analetsa lamulo limenelo . Atumiki a nthawi zonse amene akutumikila kutali ndi makolo ao , angavutike kusankha cocita . Masiku anonso Yesu amatipempha kubwela kwa iye kuti titsitsimulidwe na kutetezedwa ku zolemetsa na nkhawa za pa umoyo wathu . — Mateyu 11 : 28 , 29 . Komabe , palibe boma la anthu kapena wolamulila aliyense waumunthu amene angakwanitse kutsiliza mavuto aakulu amene ise anthu timakumana nawo . — Sal . 22 : 37 - 39 . Nditafika zaka 16 , tsiku lililonse ndinali kumwa mabotolo 10 kapena 15 a moŵa . ( a ) Pankhani yophunzitsa ena , ndi vuto liti limene akulu akukumana nalo m’maiko olemela ? Peter anayamba kuphunzila naye Baibulo . Kodi iye adzakamba ciani ? 10 : 16 ) Zimenezi zatheka cabe cifukwa ca kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova . N’cifukwa ciani Yehova amatiyang’ana ? Kodi Yesu anaonetsa kuti kupeleka misonkho tiyenela kukuona bwanji ? ( 1 Pet . 3 : 18 - 22 ) Ziukililo zoyamba zinali zocititsa cidwi , koma siziposa ciukililo capadela cimeneci . Conco , dokota savutika kucita kusakila pali mtima wa munthu wodwala . Kaŵili - kaŵili , a Loladi akapeza anthu anali kuwaŵelengela mavesi ena a m’Baibo ya Wycliffe , ndi kuwasiyila Mabaibo olembedwa pa manja . Iye sadzatiiŵala ngati ndife okhulupilika kwa iye . — Yes . Nili na makolo anga , tikuyenda ku msonkhano ku Wichita ca m’ma 1940 Tinali kugwilizana kwambili ndi atumiki a nthawi zonse , maka - maka a m’banja la Steele — Don ndi Earlene , Dave ndi Julia , komanso Si ndi Martha . Tinali kukambilana kwambili zinthu zauzimu ndipo ananilimbikitsa ngako . Kodi anakwanitsa bwanji ? N’nali kulemba ndakatulo na kucitako maseŵela a anthu olemala . Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Masiku otsiliza . . . , anthu adzakhala odzikonda , okonda ndalama , . . . okonda zosangalatsa , m’malo mokonda Mulungu . ” Kupanduka kwa mu Edeni sikunasinthe colinga ca Mulungu cimene anali naco poyamba cokhudza anthu na dziko lapansi . 12 : 5 , 6 . Ndiyeno , iye anayamba kusintha maganizo ake . Kalalikile ! N’kutheka kuti pamene anali kwawo , analibe mwayi wophunzila Baibo kapena wogwilizana ndi anthu a Yehova momasuka . Palibe cimene cikanabweletsa cimwemwe cacikulu kupambana kugwila nchito ya Ambuye kwa masiku athunthu . . . . Yehova analamula Aisiraeli kuti asadye “ magazi alionse . ” Ndinali kudziŵa kuti abale padziko lonse lapansi anali kundipemphelela . ” 17 Mmene Timavulila Umunthu Wakale ndi Kusauvalanso Mpake kuti Habakuku anafunsa kuti : “ Inu Yehova , kodi ndidzalilila thandizo koma inu osandimva kufikila liti ? ” M’dzikoli anthu amanyozela cilango ca Mulungu , ndipo amaona kuti kudzilanga wekha n’kosafunika . Yehova adzagwilitsila nchito Ufumu wa Mesiya kuthetsa mavuto a anthu . Adzacita zimenezo mwa kuononga anthu oipa ndi kupulumutsa anthu ake ku dziko loipa la Satana . ( 1 Yoh . Anakupatsani moyo , cikhulupililo , Baibo , mpingo , na ciyembekezo ca tsogolo labwino . Zimenezo sin’nade nazo nkhawa cifukwa n’nali n’tasankha kale zocita . Ena amalephela kucita zoculuka mu ulaliki cifukwa ca ukalamba kapena kudwala . Conco , pali mafunso amene nkhani ino idzayankha . Kodi Mau a Mulungu anawakhudza bwanji amuna amene anali kutsogolela ? M’kupita kwa nthawi , maneja wa pa hotelayo , dzina lake Charles Bernhardt , analandila coonadi , kugulitsa hotela yake , ndi kuyamba upainiya . Anacita upainiyawu yekha - yekha kwa zaka 15 m’madela ena akutali ndi ouma kwambili m’dziko la Australia . Ici ndiye cifukwa cake Bungwe Lolamulila likuona kuti anthu a zinenelo zonse ayenela kukhala ndi Baibulo limene limalemekeza dzina la Mulungu . Mlongo wina atasiya banja lake ndi kupita kudziko lina , anauza akulu a kumeneko kuti : “ Tinadzimana zinthu zambili kuti ndibwele kuno . Mwamuna wanga anasiya kutumikila monga mkulu . Masiku ano , Yehova amaseŵenzetsa Baibulo , mzimu wake woyela , ndi mpingo kuti atiumbe . Mwacitsanzo , nthawi zambili , oyang’anila dela amafunikila malo okhala pamene akucezela mpingo . N’zimene mtumwi Paulo anacita . Anthu mwacibadwa amafuna kukonda ena ndiponso kukondedwa . Komabe , ambili amapeleka mphatso pa nthawi ina m’caka , cifukwa congokakamizidwa kutelo . Mlongoyo anati : “ N’nali kusakila mfundo zina m’zofalitsa zathu zimene n’nali kuona monga zinganipatse ufulu woceza na mwana wanga komanso mdzukulu wathu . ” Sitiyenela kuganiza kuti wofalitsa watsopano angaphunzile luso lophunzitsa mwa kungopita mu utumiki . Monga mkulu , mungayelekezedwe ndi mlimi . Mlengalenga ndi mphamvu yokoka ya dziko zimateteza kuti kutentha kovulaza kwa dzuŵa kusaononge dziko . NYIMBO : 123 , 86 Pamafunika kukhala ndi cikhulupililo colimba kuti munthu ‘ ayende ndi Mulungu ’ monga mmene akucitila Paul ndi banja lake . ( Yes . 56 : 1 , 2 ) Ndithudi ndife odala cifukwa timakonda anzathu ndi kuwacitila zolungama . Koma pali cina cimene Yosefe anali naco . — Genesis 37 : 29 - 35 . Monga taonela , iye ali na ufulu wolamulila , ndipo ulamulilo wake ndiwo wabwino koposa . Kodi mwapindula bwanji kuphunzila Nyimbo ya Solomo ? Atatsiliza fanizolo , Yesu anagwila mau a ulosi a pa Salimo 118 : 22 . ( Oweruza 11 : 34 ) Ngakhale n’conco , Yefita anakhalabe wokhulupilika . Ndiponso palibe amene angatsutse kuti anthu ambili amafa caka ciliconse cifukwa ca matenda osiyana - siyana , masoka acilengedwe ndi milili yakupha . Machitidwe 22 : 16 Nanga imatilimbikitsa bwanji kutengela Kristu Yesu , kukonda abale athu , ndi kuwakhululukila ndi mtima wonse ? M’malomwake , tidzapitiliza kutumikila Yehova Mulungu wathu kwamuyaya tili ndi mphamvu ndiponso thanzi langwilo . Tingapitilize bwanji kuika maganizo athu pa zinthu zofunika kwambili ? 2 : 19 ) Inde , tifunikadi kukhala osiyana ndi dzikoli . Kodi timadalila malamulo a cilengedwe m’njila ziti ? Iye analemba za “ m’nyumba yaikulu ” mmene simumakhala “ ziwiya zagolide ndi zasiliva zokha ai , koma mumakhalanso zamtengo ndi zadothi . Ziwiya zina zimakhala za nchito yolemekezeka koma zina zimakhala za nchito yonyozeka . ” Zimenezi zikutikumbutsa mau a m’Baibulo akuti : “ Tangoganizani mmene kamoto kakang’onong’ono kamayatsila nkhalango yaikulu . ” Tinali kusonkhana anthu 8 . Pamene iye anali m’ndende pamodzi ndi Yosefe , analota maloto , ndipo Yosefe anamasulila maloto akewo mouzilidwa na Mulungu . Pofika kumapeto kwa zaka 1000 za ulamulilo wa Ufumu , anthu omvela adzakhala atamasuka ku adani onse amene akhalapo cifukwa ca kusamvela kwa Adamu . ( b ) Kodi anthu a Mulungu amathandizana bwanji kuti pakhale kufanana pakati pawo ? Webusaiti ya www.jw.org imakamba za “ uthenga wabwino uwu wa Ufumu . ” Motsogoleledwa ndi Yoswa , Aisiraeli anagonjetsa mzinda uliwonse ndipo anakakhala m’dziko la Kanani . Kodi ndemanga za abale aŵili zakukhudzani bwanji ? 2 , 3 . ( a ) Ni copinga citi cimene sicinatilepheletse kuwala “ monga zounikila ” ? ( Luka 19 : 2 , 8 ) Mwina , izi n’zimene okhometsa msonkho ambili anali kucita . 12 : 21 . Makolo , muyenela kuthandiza ana anu kuganizila mosamala za madalitso amene angapeze cifukwa cokhala omvela , komanso mavuto amene angakumane nawo cifukwa ca kusamvela . UMOYO NA MAKHALIDWE ACIKHIRISTU Kucokela pansi m’cigwa ca Kidroni kufika pa denga la kacisi panali potalika mamita 140 . Rahabi nayenso anacita zinthu molimba mtima . MTUMWI Paulo anakumbukila aja amene anagwila nchito yolalikila uthenga wabwino mwakhama . Panthawiyo , ine ndi Lidasi tinapemphedwa kukatumikila monga apainiya apadela ku Dómue , dela limene lili ku Mozambique pafupi ndi dziko la Malawi . Mwininyumba akaonetsa cidwi , tinauzidwa kuti tiziŵelenga malemba okamba za mmene umoyo udzakhalila mu Ufumu wa Mulungu . ( c ) ‘ maganizo athu onse ’ ? Iwo anasintha zinthu zina paumoyo wao ndi kugwilitsila nchito nthawi yao , mphamvu zao , ndi ndalama zao kuti akalalikile kumalo osoŵa . ( Yoh . 17 : 4 ) Anacita zimenezi mwa kulalikila za Ufumu wa Mulungu . Cifukwa ca kupanda ungwilo , munthu sakanaonetsa bwino - bwino makhalidwe a Mulungu . 106 : 1 ; 112 : 9 ; 117 : 2 ) Lemba la Malaki 3 : 6 limati : “ Ine ndine Yehova , sindinasinthe . ” Pofika ca m’ma 1970 , Mboni zambili ku Malawi zinathaŵa ndi kusiya katundu wao yense cifukwa cokana kuloŵa m’cipani candale . Zimene makolo ambili aona kuti n’zothandiza ndi kufunsa ana ao mafunso monga akuti : “ Umadzimva bwanji kukhala Mkristu ? Ngati mumayesetsa kuti muleke kukoka fodya koma mumalephela , musataye mtima . Iwo anali kufika kunyumba kwathu kuti aone ngati pali zina zimene tifunikila . ” Koma Yehova anali ndi maganizo osiyana . N’cifukwa ciani kuceleza abale na alongo athu n’kofunika ? Iye anatumikila Yesu mmene angathele . M’buku lake lakuti Epitome of Military Science , wolemba mbili waciroma dzina lake Vegetius ( wa m’zaka za m’ma 400 C.E . ) anakambapo za ulendo wa pamadzi kuti : “ Miyezi ina imakhala yabwino , ina imakhala yokaikitsa , ndipo ina n’zosatheka kupanga ulendo . ” Kodi munapezapo golide ? Ganizilani za Eodiya ndi Suntuke , alongo acikhiristu a m’zaka 100 zoyambilila . 12 , 13 . ( a ) N’cifukwa ciani abale 8 audindo anaweluzidwa kukapika jele zaka zambili ? Lamulo limenelo limagwilizana kwambili ndi cilungamo cake . — Salimo 37 : 28 . Komabe , Baibulo lokonzedwanso la 2013 limafotokoza kuti : “ Dzina lakuti Yehova limatanthauza zambili kuonjezela pa mfundo yakuti iye amasankha kukhala ciliconse cimene akufuna . Pambuyo pake , anafunika kuukitsidwa na thupi lauzimu monga zinacitikila kwa Khristu . Pulogalamu Yophunzila Baibulo Ya Anthu Onse 4 Ndilipo ndi moyo cifukwa cotsatila mfundo za m’Baibulo ndi kukhala ndi umoyo wacikristu . Kodi Yehova anaona kudzicepetsa kumene Ahabu anasonyeza ? Wophunzilayo ndiye anatuma foni ndi kundipempha kuti tipitile limodzi ku misonkhano . ( Aroma . 14 : 8 ) Aliyense amene wacita lonjezo la kudzipeleka afunika kuiona kuti ni nkhani yaikulu monga mmene wamasalimo anacitila . Poneza za malonjezo amene anapanga kwa Mulungu , iye anati : “ Yehova ndidzamubwezela ciani pa zabwino zonse zimene wandicitila ? Koma , bwanji ngati munthuyo wadzidziŵikitsa ndipo wakuuzani kuti amagwila nchito yofufuza zakudya zopatsa thanzi ndi kuti ali ndi mfundo zina zothandiza ? Mu 1700 C.E . , mzungu wina amene anali mtsogoleli wacipembedzo , dzina lake John Lewis analemba kuti : “ Citundu cimasila , conco n’kofunika kukonzanso ma Baibo ena akale kuti akhale na Citundu cimene anthu amakamba , cimene m’badwo umene ulipo ungamvetsetse . ” Mlongoyu anatopa , ndipo anayamba kusungulumwa . Ngakhale kuti ndinawazindikila atabwelako , sindinamasuke nao . ” Mwacitsanzo , mungakhale na nkhawa kuti mudzasoŵa cakudya . 12 : 25 ) Ngati muli ndi nkhawa , muyenela kuuzako mtumiki wa Yehova amene amakumvetsetsani . “ Musamakonda kuganizila zakuti wolakwa n’ndani nanga wosalakwa n’ndani . Jorge anatipempha kuti aziphunzila nafe Baibulo , ndipo tinavomela . Tikauza Mulungu nkhawa zathu m’pemphelo timamvako bwino . 4 : 8 ) Tizipemphela kwa Mulungu monga mmene wamasalimo anaimbila kuti : “ Tsegulani maso anga kuti ndione zinthu zodabwitsa za m’cilamulo canu . ” ( Sal . Kuonjezela pamenepa , kundikweza pa njingayo kukanapangitsa kuti kukhale kovuta kwambili kuiyendetsa . M’dziko lino limene acinyamata ambili ndi odzikonda , n’cifukwa ciani Akristu acinyamata ayenela kugwilizana ndi anthu a Mulungu ? Nthaka ikuimila mtima wa munthu wophiphilitsa . Patapita nthawi yocepa , Dorothy nayenso anakhala mpainiya . Zizindikilo zimenezi zikucitikila panthawi imodzimodzi ndi zocitika zitatu zotsatilazi . Davide anamvetsetsa mmene zimamvekela ngati ena akukupewa . — Sal . Ngakhale pamene ena anayamba kucita zinthu zoipa , Yefita ndi mwana wake anakhalabe okhulupilika kwa Yehova . Ngati asilikali azungulila mzindawo kwa nthawi yaitali , anthu mumzindawo anali kukakamizika kudya zakudya zimene anasunga . Mulungu analenga Mwana wake , Yesu , asanalenge wina aliyense kapena cina ciliconse . N’cimodzimodzinso kwa ise Akhristu “ masiku otsiliza ” ano . — 2 Tim . Kodi Yosefe anapezeka bwanji mu vuto limeneli ? Muzipempha cikhulupililo coonjezeleka . Ngati mumayesetsa kucita zimenezi , mwa dalitso la Mulungu , mungathe kuyambitsa phunzilo la Baibo . Nanga ndani anali atate ake a Yosefe ? Cikhulupililo cimaloŵetsamo zambili osati cabe kungomvetsa colinga ca Mulungu . Akadziŵa zitundu zonse ziŵili , canu na ca m’dzikolo , zimawathandiza kukulitsa luso la kuganiza , ndiponso amaphunzila kukhala bwino na anthu ena . Kodi kupilila kumatanthauza ciani ? Kukhala ndi cithunzi ca dziko latsopano m’maganizo mwathu kudzatithandiza kufuna Ufumuwo coyamba . Akuluakulu a ndende anandilamula kuti ndiwauze ciŵelengelo ca Mboni m’Malawi . “ WANDIPEZA KODI MDANI WANGA ? ” Aonekelatu kuti asunga cikhulupililo cawo colimba . Kaya ndi mmene zinthu zinalili kapena ai , cimene tikudziŵa n’cakuti vinyo unatha pa phwandolo . Mwacionekele anali kuoneka mosiyana ndi poyamba , cifukwa ngakhale anzake apamtima sanamuzindikile mwamsanga . ( Akol . Koma panthawiyo anali ataleka . Zimene ndinasankha zinali zolakwika . Kodi Kristu adzapambana bwanji pa nkhondo yolimbana ndi adani ake ? Mwamsanga , Elisa anavomela ndipo anayamba kutumikila Eliya wokalambayo mokhulupilika mwa kugwila nchito zooneka ngati zotsika . Lomba tiyeni tikambilane mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kucita “ cifunilo ca Mulungu , cabwino , covomelezeka ndi cangwilo , ” posankha zovala . — Aroma 12 : 1 , 2 . ( 2 Pet . 1 : 20 , 21 ) Conco , Baibulo ndilo mbali yaikulu ya cakudya ca kuuzimu . — 2 Tim . Cacitatu , anali ofunitsitsa kugwilitsila nchito paumoyo wao zimene anaphunzila ndiponso kuzigwilitsila nchito pothandiza anthu ena . — Mat . Moti tikhale olimba mtima ndithu ndipo tinene kuti : ‘ Yehova ndiye mthandizi wanga . Sindidzaopa . Koma ikuimila zimene zidzacitika m’masiku otsiliza a dongosolo loipa lino . Imwe acicepele , dziŵani kuti zonse zimene mumacita sizidzapita pacabe . ( Luka 11 : 2 - 4 ) Conco , palibe cifukwa congokhalila kuganizila macimo amene Mulungu anatikhululukila kale . Kwa nthawi yaitali , ndinali kulephela kubwelela kukatumikilanso abale monga woyang’anila cifukwa codziona kukhala wolephela . Nthawi zina , amacotsa ciyesoco . 34 : 29 , 30 , 33 ; 2 Akor . 3 : 7 , 13 ) Ndiyeno , Paulo anati : “ Koma munthu akatembenukila kwa Yehova , cophimbaco cimacotsedwa . ” ( 2 Akor . Amene ali pa banja akulimbana ndi mavuto ndi mayeselo ambili . ( Yes . 65 : 17 ) Kuyambila lelo mpaka panthawiyo , tiyeni tonse tiziyesetsa kucita zinthu mogwilizana ndi cilungamo ca Yehova . M’malo mokambilana zimene anthu acita kuti athetse mavuto , gwilitsilani nchito Malemba ndi kumuuza kuti Ufumu wa Mulungu udzathetselatu mavuto onse a anthu . Mwacitsanzo , ganizilani nkhani ya pa Maliko 5 : 25 - 34 . N’ciani catsatilapo pamene Mulungu walola kuti anthu adzilamulile kwa kanthawi ? Tsiku lina m’maŵa n’tatuluka panja , n’nangoona pansi ponse paoneka mbee ! M’zaka zaposacedwapa , m’baleyu anatumikila m’makomiti osiyanasiyana monga Yoona za Atumiki a pa Beteli , Yoona za Nchito Yolemba Mabuku , Yoona za Nchito Yofalitsa Mabuku , ndi ya Ogwilizanitsa . Nanga tifunika kuganizila ciani tikamaona lembali caka cino ? Vuto lina limene Nowa anakumana nalo linali lokhudza kusamalila banja lake . Ayuda okhulupilika ambili amene anagwidwa ndi a Babulo anapulumuka pamene Yerusalemu anaonongedwa , ndipo anatengedwa ku ukapolo ku Babulo . Pa Chivumbulutso 12 : 9 , Satana amachedwa Mdyelekezi , kutanthauza “ Woneneza . ” Iye anapatsa anthu oyambilila ciyembekezo cokhala ndi moyo kosatha m’paladaiso padziko lapansi . Pasanapite nthawi itali kucokela pa Pentekosite wa mu 33 C.E , mu mpingo wacikhristu munabuka vuto la tsankho . ( Miy . 24 : 6 ) Mwacitsanzo , ena angazisamalila zosoŵa zao za tsiku ndi tsiku ndipo ena angazipeleka thandizo la ndalama . Tiyeni tikambilane mmene okwatilana angalimbitsile ukwati wao mwa kuteteza mtima wao , kukhalabe paubwenzi ndi Mulungu , kuvala umunthu watsopano , kulankhulana bwino , ndi kupeleka mangawa a muukwati . Mu May 2010 , na ise tinakukila kumeneko olo kuti tinali na ndalama zocepa . ( a ) Kodi mkulu wina anathandiza bwanji wacinyamata kupita patsogolo ? KALEKALE , makhoti a ku dziko lina la azungu anakhulupilila umboni wabodza wokhudza amuna aŵili wakuti anali ndi mlandu wakupha , moti anapatsidwa ciweluzo cakuti onse aŵili aphedwe . Patapita nthawi , mpingo wacikristu unakhazikitsidwa mumzinda wa Korinto , ku Girisi . Mumzinda umenewo munali zocitika za zipembedzo zosiyana - siyana . M’caka ca 2015 cino , tikuyembekezela kulandila madalitso osaŵelengeka akuuzimu kucokela kwa Yehova . ( Sal . 73 : 28 ) Tiyeni tonse tipitilizebe kuphunzila zinthu zatsopano za Yehova . Tikacita zimenezo tidzam’konda kwambili . Apainiyawa anafikila madela ambili amene anali asanalalikidwepo . Zimene Yesu anauza ophunzila ake ocepa zingakhudzenso ophunzila ambili . Mulungu anacita zofanana ndi zimenezi m’nthawi yakale pamene anamasula Aisiraeli kucoka ku Babulo . ( Chiv . 18 : 1 - 4 ) Zimene Yehova amatiphunzitsa zimatipindulitsa . Kudziŵa zifukwa zimene Mulungu walolela mavuto kuticitikila , ndi kuti posacedwapa iye adzacotsa mavuto amenewa , kudzatithandiza kusakhumudwa ndi Mulungu tikakumana ndi mavuto alionse . Koma ca m’ma 1300 C.E . , m’pamene anapanganso makonzedwe ena akuti anthu wamba aziŵelenga Baibo m’citundu cawo . Tiyeni tikambilane mmene Mau a Mulungu amatilimbikitsila kupita patsogolo kuuzimu . ▪ Khalani Maso ! Satana Akufuna Kukumezani N’ciani cimene Baibulo limalonjeza anthu amene amasinkhasinkha Mau a Mulungu tsiku lililonse ndi kucita zimene aphunzila ? Kodi ndimakonda kukhala ndi Akristu anzanga ? ’ Baibo inakambilatu kuti “ masiku otsiliza ” anthu adzakhala “ osayamika . ” ( 2 Tim . Ganizilani izi : Aisiraeli akale anauzidwa kuti safunika kuphwanya fupa lililonse la nkhosa ya mwambo wa Pasika . Ine na Tony ndife otangwanika na nchito yoyendela ndi kulimbikitsa mipingo yosiyana - siyana ya Mboni za Yehova mlungu uliwonse . ( 2 Mbiri 22 : 9 ) Komabe , sakanapewa zotulukapo za mayanjano oipa . Baibo yamasulilidwa m’zinenelo zosiyana - siyana , koma m’kupita kwa nthawi , zinenelo zimenezo nazonso zimasintha . Iwo anacita ciwelewele . Baibulo limatiuza colinga cimene Mulungu analengela zinthu zonsezi . Abulahamu anaonetsa kuti anali kukonda Mulungu ngako , mwa kulolela kucita zimenezo ngakhale kuti anali kum’konda mwanayo . ( Ŵelengani Ezekieli 3 : 17 - 19 . ) Kodi mungawathandize motani ? Anapemphela kwa Yehova ndi kufunsila nzelu kwa Yesaya , mneneli wa Yehova . ( 2 Maf . Mitu ina ya banja imagwila nchito maola ambili kuti asamalile banja lao . VUTO LIMENE LINALIPO : Anthu otsutsa ndiponso zinthu zimene analembapo uthenga wa m’Baibulo , sizinapangitse kuti Baibulo iwonongedwe . Koma sizinathele pamenepo . Mwamuna amene amavutitsa mkazi wake kapena kum’menya amaonetsa kuti ndi wofooka , ndipo amaononga ubwenzi wake ndi Yehova . ( b ) N’cifukwa ciani acinyamata ena sanaike coonadi patsogolo m’moyo wao ? 12 Colinga ca Moyo June Koma ngakhale munthu wathu wakunja akutha , ndithudi munthu wathu wamkati akukhalitsidwanso watsopano tsiku ndi tsiku . Azimayi aŵili a Mboni za Yehova anali kubwela nthawi zonse kukaphunzitsa Baibo anzanga ena . Tidziŵa bwanji kuti kukhala na cidziŵitso ca m’Baibo pakokha , sikokwanila kuti munthu akhale wokonda zinthu zauzimu ? Pali zifukwa zambili , koma cifukwa cacikulu n’cakuti Baibo imaletsa kukhulupilila nyenyezi na kulosela zam’tsogolo . — wp18.2 , mape . Mabanja ena amene akugwila nchito yomanga ku Wallkill 5 : 2 , 3 ) Ngati Mkhristu apitiliza kusunga mfuti yodzitetezela kwa anthu , ngakhale pambuyo popatsidwa uphungu wa m’Malemba , ndiye kuti si wacitsanzo cabwino . Cilungamo cimene Mfumu ikumenyela nkhondo ndi ‘ cilungamo ca Mulungu , ’ kutanthauza miyezo ya Yehova pa zinthu zabwino ndi zoipa . ( Aroma 3 : 21 ; Deut . Nafenso tingacite cimodzimodzi . 145 : 16 ; Mat . Zikanaokabe kukhala zoona kaya Kolosase ndiye akanapambana nkhondo kapena ayi . Baibulo limalangiza Akristu kuti sayenela kukamba “ mau acipongwe . ” Koma kusankha zinthu mopanda nzelu kungaononge ubwenzi wathu ndi iye . ( Chiv . 21 : 4 ) Ambili mwa anthu amene adzaukitsidwa adzakhala “ osalungama ” amene anakhalako kalekale ndipo anafa asanaphunzile coonadi conena za Yehova Mulungu ndi Mwana wake . Iye anatipatsa moyo ndi zonse zimene tifunikila kuti tizisangalala . Ngakhalenso dokotala wanga wa zamaganizo anandiuza kuti : “ Iwe kwatha , sungapulumuke . ” Kodi tingadziŵe bwanji kuti timaona zosangulutsa moyenelela ? Kodi cikhulupililo ca Mkhiristu woona cimazikidwa pa mfundo iti ? Kunena zoona , munthu angasangalale ndi nchito iliyonse malinga ngati amaiona moyenela , kutanthauza kuti ngati amayesetsa kuiphunzila n’colinga cakuti aidziŵe bwino . Anthu ophunzitsa cisanduliko amaitsutsa mfundo imeneyi . ( Genesis 3 : 1 - 5 ) Komabe , tikaona mmene dzikoli lilili masiku ano , timaona kuti maganizo otelo amabweletsa mavuto . 58 : 13 , 14 . 24 : 14 ) Kodi uthenga wa Ufumu ‘ umagalamutsa ’ mtima wathu ? Mwacitsanzo , pophunzila za umoyo wa anthu a m’Baibulo , ganizilani zimene mungawafunse akadzaukitsidwa . Tingaphunzile zotani pa nkhani yokhudza Paulo na woyang’anila ndende ? Abale ndi alongo amenewa anacokela ku Australia , Britain , Canada , France , Japan , Korea , Spain , ndi ku United States . Ndipo ndi a zaka zoyambila pa 21 mpaka 73 . Timakondwela tikaona ciŵelengelo ca Mboni cikuwonjezeka Iye analephela kupha mfumu Agagi , mdani wa anthu a Mulungu . YEHOVA ali na cuma cambili kuposa wina aliyense m’cilengedwe conse . NYIMBO : 57 , 52 Pamene pangano la Cilamulo linali kugwila nchito , Mose ndiye anali kutsogolela mtundu wa Isiraeli . Kodi mungathandize bwanji abale ndi alongo kulimbitsa cikhulupililo cao ? Koma anakwanitsa kusintha . Mosakaikila , Paulo nayenso anakondwela kwambili . ( Ŵelengani Masalimo 49 : 7 - 9 ; 1 Petulo 1 : 18 , 19 . ) Paulo anafotokoza mmene odzozedwa amamvelela . ( Gen . 2 : 15 , 16 ) Ndipo m’zaka 100 zoyambilila , pamene mzimu woyela unayamba kugwila nchito pampingo wa odzozedwa , “ panalibe ngakhale mmodzi wonena kuti zinthu zimene anali nazo zinali zayekha . Zonse zimene anali nazo zinali za onse . ” ( Mac . Kodi milungu yako imene wadzipangila ili kuti ? Anayamba kuzonda Wycliffe , otsatila ake , ndi Baibo yake . 123 : 1 , 2 . Nanga n’cifukwa ciani mpukutuwo unali wolembedwa mbali zonse ziŵili ? 15 : 23 . Izi n’zimene n’nali kukhulupilila , ndipo n’nali kufunitsitsa kuzikwanilitsa mu umoyo wanga wonse . Iwo anakambanso kuti cikanakhala cocititsa manyazi pasukuluyo pakanakhala popanda ana a Mboni . Ganizilani cabe : Yehova analamula kuti munthu wopha mnzake mwadala , aziphedwa . Koma iye analamulanso kuti ngati munthu wapha mnzake mwangozi , azicitilidwa cifundo na kutetezedwa . Kodi Yehova watithandiza bwanji kumvela mau ake ? Mwamuna anavomeleza kuti sanali mphunzitsi wabwino komanso sanali kucititsa kulambila kwa pabanja mokhazikika . Ngakhale imfa siingathe kutilekanitsa na cikondi ca Yehova . Ndinalimbikitsidwa kwambili nditaŵelenga yankho locokela ku Bungwe Lolamulila ili : “ Sitionapo cifukwa ciliconse cimene muyenela kulekela nchito yomasulila m’Cituvalu . Mafanizo amenewa atithandiza kuona kuti kubala zipatso sikudalila mmene anthu a m’gawo lathu amalabadilila uthenga wa Ufumu tikawalalikila . Kodi kutengedwa kwawo ukapolo ndi Babulo Wamkulu kunali njila yowawongolela ndi kuwalanga ? Ndipo nthawi zambili , amayi anali kumunyamula ndi kupita naye ku cipatala , ali otsimikiza kuti wamwalila . “ Tulukani mwa iye anthu anga . ” — CHIV . Zolakwa zina zimakula msinkhu kuposa zina . Conco , tiyenela kukhala ofunitsitsa kuika pambali zokonda zathu podziŵa kuti m’dziko latsopano , Yehova adzatidalitsa ndi ‘ moyo weniweni , ’ moyo wosatha , m’mikhalidwe yacimwemwe ndi yamtendele . — 1 Tim . Tsopano tiyeni tikambilane mmene tingatengele citsanzo cake pankhani yokhala wolimba mtima ndi wozindikila . Palinso ena amene adzozedwa kuti atumikile monga mafumu ndi ansembe . Mwacitsanzo , mungapeze malangizo othandiza pa kamutu kakuti “ Mafunso Amene Makolo Amadzifunsa , ” kamene kali m’cigawo ca zakumapeto m’buku lakuti Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa — Buku Loyamba . Mfumukazi yoipa Yezebeli anatumiza uthenga kwa Eliya wakuti adzamupha . Ngakhale panthawiyo , zioneka kuti tsiku lililonse panali kutuluka zinthu zatsopano . Pamene Mose anasiya cuma ca Iguputo , anadalila Yehova . ( Aheb . KHALANI WOYAMIKILA : “ Sonyezani kuti ndinu oyamikila . ” Mwacitsanzo Danieli . Iye ndi anzake atatu — Sadirake , Mesake ndi Abedinego — anakana kudya zakudya zoletsedwa kwa Ayuda . Conco , anakuwa kuti nileke , koma sin’naleke . Mtengo umafunika madzi nthawi zonse kuti ukhale wathanzi . Nayenso Mkhristu amafunika kuphunzila Mau a Mulungu nthawi zonse kuti akhale wolimba kuuzimu . Ngati tidzipenda moona mtima ndi mwanzelu , tidzapewa kudziiunjikila maudindo ambili cifukwa codalila maluso athu . 20 : 7 - 9 ) Cikondi ca Yehova pa ana ake a mtengo wapatali n’cosatha . Lambilani Yehova , Mfumu Yamuyaya Popeza kuti hotelayo inali pakati pa tauni , ena mwa ophunzila Baibo athu anali kufuna kuti tiziphunzilila nawo Baibo ku hotelako . Yesu anacita cozizwitsa cake coyamba pa phwando la ukwati ku Kana wa ku Galileya . ( a ) Kodi kusamvela makolo , anthu ena amakuona bwanji masiku ano ? Paulo anazindikila kuti cifukwa cakuti anthu ambili m’masiku otsiliza adzakhala na cikondi cadyela , Akhristu adzakhala pa ciopsezo mwauzimu . Motelo , kaya munthu apemphele n’colinga cakuti acite bwino mayeso kusukulu , kupambana pa maseŵela ena ake , kuti Mulungu atsogolele banja lake kapena pa zifukwa zina , anthu mamiliyoni ambili amaona kuti kupemphela n’kofunika . 4 : 7 - 9 ; 1 Pet . Monga Nowa , tifunika kukhala na zocita ‘ zambili mu nchito ya Ambuye . ’ Tinakondwela kucita upainiya pamodzi . Mwacitsanzo , atayamba kulalikila mumzinda wa Kaperenao , anthu ambili anali kufuna kuti Yesu akhale nthawi yaitali mumzinda wao . Takambilananso kuti tiyenela kutengela zitsanzo zabwino za anthu auzimu . Conco , khalani odzicepetsa . Conco , n’zoona kuti Goliyati anali wamtali mamita 2.9 . Mulungu Amakuona Bwanji Kukoka Fodya ? Nthawi zokwanila 7 zinatha pamene misala ya Nebukadinezara inatha ndi kuyambanso ulamulilo wake . Koma anthu amene adzapindula ndi cikondi ca Mulungu ali ndi ziyembekezo zosiyana . Nanga tingamudziŵe bwanji Yesu ? Kodi Paulo anagwilitsila nchito fanizo lotani kuonetsa kuti sitifunika kugwilizana ndi anthu oipa ? Pokhala atumiki a Yehova , timadziŵa kuti Yesu anali munthu wapadela kwambili . Enanso amaona kuti kukhala na moyo kwamuyaya n’kotheka , koma osati pano padziko lapansi . Nthawi zina , anthu ndi makampani ena amakamba kuti apanga mankhwala ocilitsa matenda amene tikudwala . Kodi kugwila nchito yolalikila imene Yesu anatilamula n’kolemetsa ? Koma Yehova nthawi zonse amadalitsa amene amam’dalila . ” Izi zitanthauza kuti cikondi cathu pa Yehova cimaphatikizapo zimene timaganiza ndi kucita . — Ŵelengani Mika 6 : 8 . Anthu ena amasankha zinthu zolakwika . Koma Manase anacita zambili kuposa pamenepa . Zimenezi zinandikondweletsa kwambili . ” — Eziquiel , Brazil . “ Nanga ndingazigwilitsile nchito bwanji pothandiza anthu ena ? ” Cikondi cimene iye anawaonetsa sanaciiŵale . Mukatelo , mudzaonetsa kuti mumakhulupilila lonjezo la Yehova lakuti adzakuthandizani . Komabe , sizinali kuphwanya cilamulo ca Mulungu . — Mac . 21 : 18 - 27 . Paulo anacitadi zimenezi . Olo kuti iye anali wakhama pa utumiki wake , anthu ena otsutsa anali kukamba kuti ‘ iyeyo akakhala pakati pawo anali kuoneka wofooka ndipo nkhani zake zinali zosagwila mtima . ’ ( 2 Akor . pangano la Abulahamu ndi pangano la Davide . Yesu atabwela monga Mesiya , Yehova anapelekanso malangizo atsopano , ndipo anavumbula mfundo zina zambili zokhudza colinga cake . Munthu wopha mnzake mwadala nayenso anali kuphedwa na m’bululu wa munthu wophedwayo , amene anali kuchedwa “ wobwezela magazi . ” ( Num . Mungawaitaneko pa zocitika zina , ndipo zimenezi zidzawalimbikitsa . ” Tidzakambitsilana za cocitika cimeneco m’nkhani yotsatila . Patapita zaka zisanu , anatipempha kuti tikathandize mipingo ina yosoŵa kumpoto kwa England . Muzimvetsela Mau a Yehova Kulikonse Kumene Mungakhale Olo kuti anawo anali aang’ono , anali kufunsa mafunso monga akuti , “ Nikacite ciani nikadzakula ? 31 : 10 - 27 ) Funani Ufumu coyamba mwa kutengako mbali mokwanila m’nchito yolalikila ndi zocita zina zacikristu , ndipo kucita zimenezi kudzakutetezani . Akangofika , muziyesetsa kukhala bwenzi lawo leni - leni . Baibulo limatiuza kuti Debora anali “ mneneli wamkazi . ” Ngakhale kuti timaitanidwa nthawi zonse kuti tidzadye “ patebulo la Yehova , ” sitiyenela kuona mwai umenewu mopepuka . — 1 Akor . Mumzinda wina wa ku Indonesia , abale anaitana akuluakulu a boma ndi anthu ena kuti adzaone Nyumba ya Ufumu yatsopano ikalibe kupelekedwa . Yesu sanaonetse kuti zimene anthu ananenela mtumikiyu zinali zoona kapena zabodza . M’malo mwake , monga anthu a Yehova tiyenela kupewelatu ampatuko . Kumathandiza munthu kukhala na maganizo abwino komanso kudzimva kuti ali pa ubwenzi wabwino na Mulungu Ngakhale n’conco , anthu ambili m’dzikoli amakonda kwambili ndalama na zinthu zakuthupi . ( b ) N’cifukwa ciani sitiyenela kuyopa kupemphela mokweza mau kwa Yehova ? N’ciani cingatithandize kukhala paubwenzi ndi Yehova ? Iwo anali okhumudwa ndi zimene zinacitika , ndipo sanadziŵe kuti Yesu waukitsidwa . Mwacitsanzo : Kodi anthuwo ali pa cibwenzi ? 17 : 1 . Coyamba , muyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi nkhani imeneyi yacokela pa webusaiti yodalilika ? 6 : 17 - 22 ) Kodi zimenezi zinapangitsa kuti ubwenzi wa Gidiyoni ndi Mulungu usokonezeke ? Nanga tingacite bwanji zimenezo ? Muzilola Yehova kuti adzikutsogolelani musanapange zosankha , osati mutasankha kale . Pamene ndinali kukwanitsa zaka 17 , ndinali nditaloŵako kale m’ndende . * Ngakhale kuti panthawiyo kunali citsutso coopsa , msonkhanowo unayenda bwino . 3 : 10 - 12 . Robert Wallen Imfa nayonso idzatha . Zimakhala zovuta kudziŵa kuti uthenga wa Ufumu wafika pati m’maiko amenewo , koma tingadabwe tikaona zotsatilapo zake . Ngati mu mpingo mwanu muli ofalitsa amene anabwela monga otumikila kosoŵa , muzicita zinthu zoonetsa kuti mumawakonda . Atumiki a Mulungu ambili amakono , naonso aonetsa cikhulupililo mwa Yehova ndi kucita zinthu moyenelela . Makolo afunika kukhala na colinga cothandiza mwana wawo kuti adzakhale wophunzila wa Khristu ( Onani palagilafu 16 , 17 ) Ndipo adzakhalapobe nthawi zonse mpaka muyaya . Tikacita zinthu modzikweza , coyamba timalephela kulemekeza Yehova monga Mfumu yathu . Kusintha kumeneku kwathandiza mabanja a Beteli kukhala ogwilizana kwambili . Tinayenda maulendo ambili kupita ku positi ofesi kukatenga mabokosi a magazini ndi kuwabweletsa kumene tinali kukhala . Kuganizila cikondi ca Mulungu kungatilimbikitse bwanji kukhala wodzicepetsa ? Palibe munthu ndi mmodzi yemwe amene anamuonapo kapena amene angamuone . ” Ndinazoloŵela kuŵelenga kucoka kumanzele kupita kulamanja , koma anthu a ku Japan amakonda kuŵelenga malembo amene amayambila pamwamba kupita pansi . ” Makolo ena amene anapita kukakhala ku maiko ena amatumiza ana awo akhanda kwa abululu ŵawo kuti akaŵasamalile . Amacita izi kuti apeze bwino mpata wogwila nchito ndi kupanga ndalama m’dziko lacilendo . 1 : 27 ; 2 : 15 - 17 ) Nayenso mtumwi Yohane anati : “ Aliyense amene ali ndi zinthu zofunika pa moyo , n’kuona m’bale wake zikumusoŵa , koma osamusonyeza m’bale wakeyo cifundo cacikulu , kodi munthu ameneyu amakonda Mulungu ? ” ( 1 Yoh . Mnyamata wina dzina lake Samuel anati : “ Cinali cosavuta kuyamba cizoloŵezi cokopana . Cifukwa cakuti Aisiraeli anapanduka , Mulungu analola kuti agonjetsedwe ndi Ababulo mu 607 B.C.E . Nkhani izi zidzayankha mafunso aya : N’cifukwa ciani olambila Yehova ayenela kucita zinthu mwadongosolo ? Mau athu angakhudze kwambili anthu ena . ( Aroma 12 : 21 ) Mpainiya wina , dzina lake Jessica , anati : “ Nthawi zambili nimakumana ndi anthu odzitukumula , amene amatinyoza komanso kusuliza uthenga wathu . Dama . Odzozedwa okhulupilika akhala akutsatila cenjezo limenelo ndi kucita khama kuti apitilizebe kukhala maso . Kenako iye anayankha kuti , ‘ Mulungu adzatelo kudzela mwa Yesu Kristu Ambuye wathu . ” — Aroma 7 : 14 , 24 , 25 . Yesu anakamba kuti : “ Amene adzapilile mpaka pa mapeto , [ mapeto a moyo wake kapena a dongosolo loipa la zinthu ] ndiye amene adzapulumuke . ” Kupatsa mwanjila imeneyi kumawapindulitsa m’njila zambili , ndipo phindu lalikulu n’lakuti matupi awo amakhala athanzi . Tikupemphani kuti muŵelenge nkhani ziŵili zotsatila kuti mudziŵe mayankho a m’Baibo pa mafunso amenewa . Yesu anakamba kuti kukonda anzathu , komwe ni mbali ya cikondi ca a·ga’pe , ndi lamulo laciŵili lalikulu kwambili m’Cilamulo ca Mose , ndipo loyamba ni kukonda Mulungu . Pocita kulambila kwa pabanja kapena phunzilo la umwini , mungayese kucita izi : Tengani buku lanu la nyimbo na kusankha imodzi mwa nyimbo zimene mumakonda kwambili . Ndipo khalidwe lathu loyela liyenela kuonetsa kuti timayamikila kwambili magazi a Yesu opulumutsa moyo . Monga anthu ambili ku Japan , ndinakulila m’banja la cipembedzo ca Cibuda . Pofuna kutithandiza , Mulungu amagwilitsila nchito mabwenzi ake okhulupilika , monga mmene Eliya analili , kuti atipatse malangizo ake . Mfumu yoikidwa ya Yehova , yakhaladi ikulinganiza nzika za Ufumu kuti zizicita zinthu mogwilizana ndi njila za Mulungu . Conco , ngati munthuyo wacita chimo lalikulu , adzayankha mlandu kwa Yehova ndi ku mpingo . ( Luka 23 : 46 ) Yesu popemphela kwa Atate wake wakumwamba , amene ndi “ Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi , ” anapeleka citsanzo cabwino kwa onse cofunika kucitsatila . Pamene mukuvutika cifukwa ca ciyeso , muziyesa kuona izi m’maganizo mwanu . Ngati n’conco , dziŵani kuti cikhulupilo ca Davide sicinali ngati maloto cabe koma cinali na maziko ake . ( Mateyu 28 : 19 , 20 ; 1 Petulo 3 : 21 ) Mukabatizidwa , mumasonyeza kuti munalonjeza kuti mudzatumikila Yehova kwamuyaya , ndipo muyenela kusunga lonjezo lanu . 5 : 3 ) Ponena za cibadwa ca anthu cofuna kulambila , buku lina lochedwa Man Does Not Stand Alone , lombedwa ndi A.C . Morrison linati : “ Tiyenela kucita mantha , kudabwa ndiponso kupeleka ulemu poona kuti anthu kulikonse amafunafuna wina wake wapamwamba kwambili ndi kum’khulupilila . ” Timadziŵa bwanji kuti kufunafuna Mulungu si kopanda phindu ? Kodi kufunafuna Mulungu n’kopanda phindu ? Jowana ndi amai ena ambili , anali kutumikila Yesu ndi atumwi “ pogwilitsa nchito cuma cao . ” Komanso cinyengo m’zipembedzo cidzaculuka . Pofotokoza ulosi wa pa Chivumbulutso caputala 17 , M’bale Knorr anapeleka umboni wosonyeza kuti padziko lapansi padzakhala mtendele pambuyo pa nkhondoyo . — Chiv . Kodi makolo athu oyambilila anacita bwanji na lamulo limenelo ? Anthu anali kukamba zabodza ponena za Yesu . Ndipo iye anauza ophunzila ake kuti adani ao adzawazunza ndi ‘ kuwanamizila zoipa zilizonse . ’ Iye anali ataloŵeza nkhani yake yonse pamtima . ( Lev . 9 : 1 - 4 , 15 - 21 ) Nsembe zimenezo zinayenela kukhala zopanda cilema cifukwa zinali kuimila nsembe yangwilo ya Yesu . Ukapolo wa ku Babulo unali wosiyana kothelatu na ukapolo wa Aisiraeli ku Iguputo zaka zambili kumbuyoko . — Ŵelengani Ekisodo 2 : 23 - 25 . Kodi mukanaleka kutumikila Yehova ? Mwana wamkazi wa m’banjalo , dzina lake Sakiko , anakamba kuti : “ M’zaka za m’ma 1990 , kaŵili - kaŵili tinali kukumana ndi anthu ocokela ku Brazil tikakhala mu ulaliki . Onani mmene akulabadilila coonadi ca m’Baibo . ’ Anali kuweluza ena mwamsanga . Pamene nthawi inafika yakuti Yesu ayambe kulamulila monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu kumwamba , Yehova anathandiza anthu kudziŵa nthawi ya zocitika zimenezo . Ndiyeno , ndinazindikila mmene ndingagwilitsile nchito cinenelo kutumikila Yehova . Mu Yudeya monse munali makhoti ang’ono - ang’ono . Ambili mwa anthuwa sadziŵa zambili za Cikristu . Abale ndi alongo omwe ndi mbeta ndi otsimikiza mtima kukondweletsa Yehova , ndipo amafuna kukwatilana ndi munthu amene amalambila Mulungu . Yesu anaphunzitsa ophunzila ake kuti sayenela kulola zinthu zambili kuwasokoneza , monga mmene anauzila Marita mokoma mtima . [ 2 ] ( palagilafu 15 ) Kuti mudziŵe zocita ngati Mkhiristu aona kuti m’pofunika kupeleka Mkhiristu mnzake kukhoti , onani buku lakuti “ Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu , ” tsa . 223 . 1 : 7 ) Pa kacisi , Ayuda anayamba kucita ciwawa , ndipo anafuna kupha Paulo . Yakobo sanagogomeze kuti munthuyo anakonza zolakwika zake mwamsanga kapena kuti anakonza zolakwika zonse . M’malo mwake , Yakobo anakamba kuti munthuyo ‘ analimbikila kutelo m’lamulo langwilo . ’ Tingagonjetse bwanji zopinga zimene zingatilepheletse kukhala oceleza ? Kodi Yehova anasonyeza bwanji kuti anali wokhulupilika kwa bwenzi lake Abulahamu ? “ Mudzaimilile cilili ndi kutukula mitu yanu , cifukwa cipulumutso canu cikuyandikila . ” — LUKA 21 : 28 . Komabe , Mulungu angatithandize kukula kuuzimu mwa kulola kuti tiyesedwe ndi zinthu zovuta . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene cikhulupililo cinathandizila Mose kuona “ Wosaonekayo . ” — Aheb . Yehova watiphunzitsa mmene tingaonetsele cikondi : Yehova samangotiuza kuti amatikonda , koma wacita zinthu zambili zoonetsa kuti amatikondadi . ( Yoh . 13 : 21 - 27 ) M’munda wa Getsemane , Yesu molimba mtima anadzidziŵikitsa kwa asilikali amene anabwela kudzam’gwila . ( Ŵelengani Salimo 122 : 3 , 4 . ) Mwa zocita zathu . Popeza Bungwe Lolamulila ni lopanda ungwilo , pakubuka mafunso ati ? Munthu Amene Mukonda Akadwala Matenda Osacilitsika , Na . Ngati iye sali paubwenzi wabwino ndi Yehova ndipo ndi wosakhulupilika , koma wadya mkate ndi kumwa vinyo , ndiye kuti wacita zinthu mopanda ulemu . Podzafika mu 1919 , nchito yolalikila ‘ uthenga wabwino wa Ufumu ’ inapita patsogolo kwambili . Samalani ndi Anthu Ogwilizana Nao Masiku Ano Otsiliza Iye anazindikila kuti kubwela kwa Khiristu kudzakhala kosaoneka , ndi kuti “ nthawi zoikidwilatu za anthu a mitundu ” zidzatha mu 1914 . Conco , ndinawapempha kuti akandilembele cabe malemba okhudza ciphunzitso cacikatolika ca kuloŵana m’malo kwa atumwi . Ndizibwela kukuthandiza . ” 3 Mbili Yanga Kusiilana Citsanzo Cabwino Komanso sakanakhala zitsanzo zabwino pankhani ya cikhulupililo colimba kwa anthu mamiliyoni ambili . Iwo adzaona kuti Mulungu amene timalambila ndi woyela ndi kuti posacedwapa adzasintha dzikoli kukhala paladaiso wokongola . — Yes . ( Yohane 5 : 28 , 29 ) Kumeneko iwo savutika kapena kumvela kuŵaŵa kulikonse , cifukwa “ akufa sadziŵa ciliconse . ” Masiku ano , maganizo a anthu m’dzikoli komanso zocita zao , n’zofanana ndi za Akanani . Mngeloyo anapitiliza kuuza mneneli Danieli kuti : “ Udzauka kuti ulandile gawo lako pa mapeto a masikuwo . ” Iye anasangalala kuti Atate wake anavomeleza kaphunzitsidwe kameneko . Nthawi yoyamba pamene n’namvela za ciphunzitso ca Utatu , n’nali na zaka 12 . 8 : 4 , 7 ) Imeneyi inali nkhani yodetsa nkhawa , ndipo ikanatha kugaŵanitsa mpingo . Tumikilani Yehova ndi Mtima Wathunthu , Mar . Zikakhala conco , tingakhale okondwa pozindikila kuti sitinakulitse nkhaniyo mwa kuipitsa mbili ya Mkhristu mnzathu . Pamene Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse inali kufalikila m’madela ambili ku India , n’nayamba kukumana na mavuto ambili mu umoyo wanga . Atatsala pang’ono kufika pamene panali ife , anazindikila mbala imene akuluakulu a boma anali kuifunafuna . ( 2 ) Tingacite ciani kuti tikhale munthu wauzimu na kupitilizabe kupita patsogolo monga munthu wauzimu ? Nthawi zina , kupanga zosankha kumawavuta . Ndi liti pamene pangano latsopano linayamba kugwila nchito ? Kodi anthu anakhudzidwa motani ndi nkhondo yoyamba ya padziko lonse ? M’malo mwake , imathandiza mkazi kukwanilitsa mbali imene Mulungu anam’lengela pamene anati : “ Si bwino kuti munthu [ Adamu ] akhale yekha . Koma kodi n’ciani cimene Anna anali kucita ngakhale pamene anali na zaka 84 ? Mboni ina imene yatumikila kwa zaka zambili inachula cifukwa cake imakhulupilila coonadi cimene timalalikila . Inati : “ Kuphunzila kwanga Baibulo zaka zonsezi , kwandithandiza kukhulupilila kuti Mboni zimayesetsa kwambili kutsatila citsanzo ca Akristu a m’nthawi ya atumwi . N’ciani cidzatithandiza kukhulupilila kuti Yehova amatikonda ? Ndi funso liti limene ena angafunse ? Kumbukilani kuti Mulungu analenga angelo na mphatso ya ufulu wosankha . ( Sal . 147 : 6a ) Koma kodi tingacite ciani kuti iye azitithandiza ? Colinga cathu cinali kukhala mu botilo ndi kuligwilitsila nchito pozungulila dziko lapansi lokongolali . Pansi pa kamutu kameneka pali funso ndi malemba amene tingakambilane paulendo wobwelelako . Monga takambila kale , cioneka kuti mitundu yonse iŵili ya ma IUD imasintha zinthu zina mkati mwa cibalilo . N’ciani cidzaloŵa m’malo mwa mabungwe acinyengo ? Tingacite ciani kuti tipindule mokwanila na cilango ca m’Malemba cimene tingalandile mu mpingo ? ( 2 Pet . 3 : 3 , 4 ) Conco , pokweza ucifumu wake , Yehova adzaonetsetsa kuti wapulumutsanso anthu onse omvela . 10 : 32 , 33 ; 13 : 4 , 5 . * Munthu wa cikondi cimeneci amaonetsa kuti amatsatila mfundo zapamwamba . Mwacionekele , Marita anamvelapo za cocitika capadela cimeneci . Yesu Kristu anakamba kuti : “ Tsopano maziko opelekela ciweluzo ndi awa , kuwala kwafika m’dziko koma anthu akonda mdima m’malo mwa kuwala , pakuti nchito zao n’zoipa . ” Ndi kusintha kotani kumene ophunzila oyambilila a Kristu anakhala nako ? Dzina , Na . Akulu - akulu kumeneko anan’tumiza ku sukulu yapamwamba ya maphunzilo a usilikali cifukwa coona kuti n’nali na luso lokhala mtsogoleli wabwino . Atsogoleli acipembedzo Aciyuda anapanga malamulo awo okamba za mocitila ndi akhate , amene m’Malemba mulibe . Malamulo amenewa anapangitsa kuti anthu odwala khate azivutika kwambili . N’ciani cinacitika pa Pentekosite wa mu 33 C.E ? Nanga ndani anakhala mtundu watsopano wa Yehova ? Kumeneku ndi kuyelekezela kwabwino . ( Zef . 1 : 14 ) Mau aulosi ocenjeza amenewa akhudzanso ise masiku ano . Ndipo zandithandizanso kuti ndiziwalemekeza monga atate ndi mutu wa banja wa kuuzimu . ” 13 : 11 - 24 ( Chivumbulutso 19 : 11 - 21 ) Kukamba zoona , atsogoleli a machalichi acikristu sadziŵa zimene Yesu adzacita monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu . Kodi zimenezi zikutanthauza kuti odzozedwa ‘ adzakwatulidwa ’ kupita kumwamba ndi thupi la nyama ? Inde , Akhiristu ali pabanja amene satayana ndi anthu a Yehova , amene amagwilitsila nchito uphungu wa m’Malemba , ndi kulola mzimu woyela wa Yehova kuwatsogolela , akhoza kusunga “ cimene Mulungu anacimanga pamodzi . ” — Maliko 10 : 9 . Iye anati : “ Ndinetu kapolo wa Yehova ! Iwo anacha mkate umenewu mana , * ndipo anaudya kwa zaka 40 . — Ekisodo 16 : 4 , 13 - 15 . ( Salimo 2 : 8 , 9 ; Chivumbulutso 16 : 14 ; 19 : 19 - 21 ) Cimodzi mwa zinthu zimene Ufumu wa Mulungu udzacita n’cakuti udzathetsa maboma onse a anthu cifukwa amacita ziphuphu . 3 ‘ Pitilizani Kukonda Abale ’ Koma ngati mumalanga ana mwacikondi ndi modziletsa , mungakhale ndi zotsatilapo zabwino . Nanga kuti tisunge malonjezowo , tifunika kuwaona bwanji ? N’zoona kuti Mulungu sindiye anacititsa kuti Baibulo ligaŵidwe kukhala m’macaputala ndi m’mavesi , ndipo nthawi zina ziganizo zina zimamveka monga zikuimila panjila cifukwa ca mmene mavesi kapena macaputala anakhalila m’Baibulo . M’nkhani zonse ziŵili , tidzakambilana maumboni atatu oonetsa kuti zoona Yehova anali kucilikiza amunawo . Izi zionetsa kuti ndiye anali kuwatsogolela , ndi kuti akali Mtsogoleli wa anthu ake . — Yes . Nanga mwaganizilapo zimene mudzacita pa umoyo wanu ? 1 : 2 , 16 ; Luka 3 : 23 , 34 . Kodi Mkhristu angafunike kuleka ciani kuti Mulungu apitilize kumucitila cifundo ? Koma Yehova anapeleka malangizo osiyana . Umu ni mmenenso zinalili m’zaka 100 zoyambilila . 9 : 27 ) Motelo , kuti tikhalebe pa mpikisano wokalandila moyo , tiyenela kusamala ndi zimene timacita . Papita zaka , Mulungu anathandizanso akazi a makolo akale okhulupilika amene anali kuopa Yehova . Zinthu zimenezi zimakhala za kanthawi kocepa , ndipo posapita nthawi zikhoza kuiŵalika . ( Genesis 12 : 2 - 4 ) Pamene anali kusamuka ku Harana , Abulahamu anali na zaka 75 , ndipo Sara anali na zaka 65 , koma analibe mwana . Pofika zaka za m’ma 1400 C.E . , zigawo za Baibulo ziyenela kuti zinali zitamasulidwa kale m’zinenelo 33 . Pambuyo pa nkhondo yaciŵili ya pa dziko lonse , Gleissner mobweleza - bweleza anagwilitsila nchito udindo wake kuthandiza Mboni za ku Austria . mu Galamukani ! ya September 2011 [ Cithunzi papeji 25 ] Iwo amakamba kuti popeza dziko likupita patsogolo m’zolankhulila , zinthu padzikoli zikuoneka kuti zikuipilaipilabe . ( Akol . 4 : 16 ) Kodi tingakambe kuti cakudya cathu ca kuuzimu n’cosakwanila , cabe cifukwa cakuti tilibe kalatayo ? Kenako ndinamva mau ngati ocokela pakati pa zamoyo zinayi zija . M’pake kuti Mboni za Yehova zimapeleka ulemu woyenelela kwa olamulila a boma mogwilizana ndi cikhalidwe ca kumaloko . Tsopano , Mboni za Yehova zimafalitsa mabuku ofotokoza Baibulo m’Cikatalani . Ndipo anthu acikatalani apindula ndi misonkhano ya mpingo m’cinenelo cao . ( b ) Ndi mwai waukulu uti umene tonse tili nao ? 11 , 12 . ( a ) Tumapepala twauthenga tungathandize motani kuti ulaliki wanu ukhale wokondweletsa ? M’buku limeneli muli ulosi wazoona wa Inoki , koma cioneka kuti mau a ulosi amenewa anatengedwa ku zolemba zakale zimene masiku ano kulibe , kapena ku nkhani zimene anthu anali kukamba . Iye anakonza pulogilamu yophunzitsa anthu poseŵenzetsa “ buku la cilamulo ca Yehova . ” Kucokela nthawiyo , anthu aona kukwanilitsidwa kwa mau ouzilidwa awa : “ Tsoka dziko lapansi ndi nyanja , cifukwa Mdyelekezi watsikila kwa inu , ndipo ali ndi mkwiyo waukulu podziŵa kuti wangotsala ndi kanthawi kocepa . ” — Chiv . Lembali limati : “ ‘ Inu ndinu Mboni zanga ’ akutelo Yehova ‘ ndipo ine ndine Mulungu wanu . ’ ” Tinafunsanso kuti : “ Bwanji ponena za Utatu ? Komabe , miyezi yocepa io asanamwalile anaona kuti anacita bwino kuvomela kukakhala kunyumbayo . ” Mwa ici , udzakhala na cikhulupililo cokuthandiza kulimbana ndi zimphepo za ciphunzitso conama . — Yer . Koma kodi pali cinacake m’thupi mwathu cimene cimapitiliza kukhala na moyo tikafa ? Anthu ena pofuna kukhala okhulupilika ku mtundu wao amapikisana , kudana ngakhale kuvulazana ndi kuphana . M’kupita kwa nthawi banja lonse linabatizika . Tiyeni tikambilane zitsanzo zingapo . Sin’naphunzile kukhululukila ena . Komabe , makolo ambili masiku ano savomeleza miyezo ya m’Baibulo ya cabwino ndi coipa . Uphungu umene anali kundipatsa pambuyo pokamba nkhani unandithandiza kuti ndikhale mkambi wabwino . Machitidwe caputa 7 - 9 , 13 - 28 Motelo , inenso nifunika kutumikila kumene aniuza . ” ( Aef . 4 : 1 ; Afil . 1 : 7 ; Filim . Ndipo monga mmene tidzaphunzilila kutsogoloku m’phunzilo lathu la Baibulo , tidzaona kuti maumboni onse aonetsa kuti tikukhala m’nthawi imeneyo . Baibulo limatilangiza kuti ngati timakwiya msanga , tidzayamba kukangana kwambili ndi anthu ndipo tidzacita macimo ambili . — Miyambo 29 : 22 . N’nali kusangalala kwambili ndi utumiki kumeneko cifukwa tinali kuseŵenza ndi anthu ambili anzelu . Baibo inalembewa kuti itipindulitse . Ngakhale kuti abale okhulupilika amenewa anali ndi atumiki ena amene anali kuwathandiza , m’bale mmodzi ndi amene anali ndi udindo wopanga zosankha kaya ndi pa mpingo , pa nthambi kapena ku likulu lathu . Maulosi a m’Baibulo amaonetsa kuti Ufumu wa Mulungu udzabwela posacedwa . — Mateyu 24 : 3 , 7 , 12 . M’malo molankhula mau ofooketsa ngati awa , Akristu ayenela ‘ kukumbutsa akazi acitsikana kukonda amuna ao , kukonda ana ao . . . kugwila nchito pamakomo ao , ’ “ kuti mau a Mulungu asanyozedwe . ” — Ŵelengani Tito 2 : 3 - 5 . Ndimafuna kuwathandiza kukhala ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha m’dziko latsopano mmene simudzakhala cinyengo . — Salimo 37 : 10 , 11 . Ndipo zimenezi zinalidi zoona , cifukwa Ophunzila Baibulo a kumeneko modzipeleka anasunga ndi kudyetsa abale ndi alongo ao akuuzimu . Ndipo analekadi . Ndiponso , kupatsa kungacetseko nkhawa ndi matenda a BP . Popeza mwana m’banjali n’nali nekha , n’nali kusoŵa munthu wonitonthoza na kunilimbikitsa . 24 : 3 , 21 , 29 ) Ndipo cosangalatsa n’cakuti “ khamu lalikulu ” la anthu lidzapulumuka cisautso ca padziko lonse cimeneco . M’bale Mumba : Pali zifukwa zambili zimene anthu amanenela conco . 4 : 8 - 11 ) Timaonetsa kuti timafuna kukhala “ ana a Atate [ wathu ] wakumwamba ” mwa kukonda mnansi wathu . ( Mat . Mapulaneti na nyenyezi zilibe mphamvu yotsogolela umoyo wa anthu , monga mmene okhulupilila zakuthambo amakambila . 6 : 7 ) Anthu ambili analandila coonadi atalalikilidwa ndi gulu latsopano limenelo . Hans anati : “ Tinali kusangalala kwambili ndi utumiki cakuti tinawonjezela masiku okhala kumeneko . ” Panthawiyo , pakhomo tinatsala cabe na mwana wathu wamwamuna wothela , Vitaly . 2 , 3 . ( a ) Kodi cikhulupililo cathu n’cofunika bwanji ? AKULU aŵili anaitana Fernando * kuti akambe naye pambali . * Madokota anakamba kuti mwamuna wake adzangokhala miyezi yocepa , ndipo adzamwalila . Monga mmene taonela , kukonza cipulumutso cathu ni udindo waukulu . Masiku ano , anthu otsutsa amaitana Yaeli ndi maina oipa osiyanasiyana . Monga mmene taonela kwa acicepele amene tawagwila mau m’nkhani ino , palibe cifukwa comuyopela Satana na ziŵanda zake . Araceli Mafunso a conco angatithandize kucitila mwininyumba aliyense zimene afuna . Poyamba , colinga ca M’bale Russell cinali kudziŵa machechi amene anali kuphunzitsa coonadi . Caciŵili , Yehova satiteteza ku “ nthawi yatsoka ndi zinthu zosayembekezeleka . ” Ndipo anawakakamiza kuloŵa nchito ya usilikali . Tiyeni tione zimene zinacitika kuti mkazi woyamba , Hava , ayambe kulakalaka kudya cipatso coletsedwa ca “ mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa . ” ( Gen . Priscilla nthawi zambili anali kukumbukila mau a Yesu a pa Mateyu 6 : 34 . Koma poona kuti panalibe “ nyumba , ” kapena kuti kacisi wopelekedwa kwa Yehova , iye anafuna kum’mangila . Conco ananitumiza ku Athens kuti nikazengedwe mlandu m’khoti ya asilikali . Kumeneko , anagamula kuti nikhale m’ndende zaka zitatu . Nkhaniyi idzafotokoza maumboni atatu amene amathandiza Akristu kukhulupilila kuti Ufumu wa Mulungu udzaononga dongosolo loipali posacedwapa . Kodi dziko limaoneka bwanji ? 9 : 23 - 25 ; 10 : 1 ) Zimakhala zocititsa cidwi ndi zolimbitsa cikhulupililo kuphunzila nkhani zokhudza ulosi zimenezi . Akhristu amalemekeza cikumbumtima ca ena . Munthu wolungama ameneyo anali ‘ kuvutika mtima kwambili ’ cifukwa ca khalidwe lotayilila la anthu a m’mizinda ya Sodomu ndi Gomora . 18,646 Timalakalaka nthawi pamene matenda na ukalamba zidzasila . Kodi Mulungu adzacita ciani kuti aononge adani athu amenewa ? Potsatila citsanzo ca Yehova , kodi tingawathandize bwanji anzathu ? Paulo anauza abale a mu mpingo wa ku Filipi kuti , ‘ [ Timoteyo ] adzasamaladi za inu moona mtima . ’ ( Afil . ( Aefeso 5 : 15 , 16 ) Koma pali cizoloŵezi coipa cimene tiyenela kuyesetsa kupewa . Mwacitsanzo , mungathandize wina wake mwa kudzipeleka kum’gwilila nchito zina zapakhomo , kapena kukam’gulila zinthu kumsika . — Mat . Pambuyo popambana nkhondo imeneyo , mfumuyo idzakwatila mkazi wokongola kwambili . Yehova anapatsa Adamu ndi Hava lamulo losavuta kulitsatila , kuti aone ngati iwo anali kuzindikila malile a ufulu wawo . Koma pamene mfumu Nero anamwalila mu 68 C.E . , Vespasian anabwelela ku Roma kukakhala mfumu . Pulogilamu yogonjetsa Yudeya , anaisiila mwana mwake Tito , pamodzi na gulu la asilikali pafupi - fupi 60,000 . 3 : 17 , 18 . N’ciani cingatithandize kuti tiziona zosangulutsa moyenelela ? Acicepele amenewa amasangalala kwambili na umoyo wawo , ndiponso amayesetsa kutsatila citsogozo ca Yehova pa zosankha zawo zonse , kaya zokhudza maphunzilo , nchito , na banja . 3 : 2 ) Koma kodi timaleka kukamba cifukwa ca zimenezi ? M’bale Otto Kuglitsch , amene akutumikila ndi mkazi wake , Ingrid , ku ofesi ya nthambi ku Germany , anali katswili pa nchitoyi . Kodi atumiki a Yehova amalimbana ndi ciani ? Iye anati : “ Nthawi ina , n’navutika ngako na nkhawa cifukwa coganizila zimene zinanicitikila kale komanso mavuto ena . Ngakhale n’conco , io anaona kuti Yehova amawakonda ndipo anali kuwasamalila . 13 , 14 . ( a ) M’nyimbo imene Aisiraeli anaimba , kodi analengeza ciani ponena za ulamulilo wa Yehova ? Mphunzitsi wina ataona mmene ndinali kugwilila nchito anakamba kuti : “ Tidzakuphunzitsa kupanga sopo . ” Kaŵili - kaŵili Baibo imakamba kuti Mulungu adzacotsa imfa ndi kubweletsa moyo wosatha . — Onani bokosi lakuti , “ Kugonjetsa Imfa , ” m’nkhani ino . Yesu anafotokoza kuti : “ Mthandizi , amene ndi mzimu woyela , amene Atate wanga adzatumiza m’dzina langa , adzakuphunzitsani zinthu zonse . ” 112 : 1 , 3 ) Conco , khalani otsimikiza mtima kutsatila lamulo la Mulungu lokhudza kukwatiwa “ mwa ambuye . ” Tidziŵa cifukwa Yehova analenga anthu m’cifanizilo cake , ndipo tonse tingathe kutengela makhalidwe ake abwino . — Gen . Ndipo anthu amene mnzawo wa m’cikwati wamwalila , mwamsanga cisoni cawo cimacepako ngati athandiza ena . Mdzukulu wa Abulahamu Yakobo , kapena kuti Isiraeli , anali ndi ana 12 . Conco , anchito ambili amadandaula kuti amasoŵa owalimbikitsako . 2 : 4 . A Daka : Inde ndamva anthu ambili akulichula ndipo mau ake amapezeka pa zizindikilo ndiponso pa zikwangwani . Muzisangalala ndi nchito iliyonse imene mumagwila ngakhale ndi yaing’ono . Ngati tikhulupilila Yehova kwambili , tidzayambanso kum’konda kwambili VUTO : Dyela ndi kudzikonda n’zimene zimacititsa kuti anthu azicita ziphuphu . Yehova atamandike potilola kudzatumikila kuno . ” Komabe , Yehova anali atawacenjezapo kale izi zisanacitike . — Eks . Ngakhale acite cidwi ndi zimene Baibulo limaphunzitsa , ena saona kufunika kophunzila nafe Mau a Mulungu . ( Ŵelengani Yohane 18 : 33 - 37 . ) Patapita zaka , anapempha mkulu amene anali kugwilizana naye kuti aziphunzila naye Baibo . ( Chiv . 18 : 8 , 21 ) Anthu akufa adzaukitsidwa ndi kupatsidwa mwai wokhala ndi moyo wosatha . ( Yes . 25 : 8 ; Mac . Zimenezi zinacitika zaka 125 Yerusalemu asanaonongedwe mu 607 B.C.E . ( 1 Mbiri 29 : 9 ) Tiyeni na ise tipitilize kupeza cimwemwe mwa kupatsa Yehova zinthu zocokela m’dzanja lake . kukamba mokoma mtima ? Tica wina anati : “ Ana onse akanakhala ngati anu , sembe nchito yophunzitsa siivuta . ” ( Agalatiya 2 : 20 ) N’zoona kuti Yesu anafa Paulo asanakhale Mkristu . Komanso mlongo wina wosakwatiwa anathedwa nzelu pamene nyumba yake inaonongeka ndi cimphepo camkuntho . Yehova anauza Aisiraeli kuti sadzalephela kukhala ndi wosauka m’dziko lao . ( Deut . Timaŵelenga kuti : “ Koma Mulungu anauza Abulahamu kuti : ‘ Usaipidwe ndi ciliconse cimene Sara wakhala akunena kwa iwe cokhudza mnyamatayo ndiponso kapolo wakoyo . Mapili a Teskey Ala - Too ( Ŵelengani Salimo 95 : 8 , 9 . ) M’modzi wa iwo anali msilikali , dzina lake Sadiq Masih . Iye anali kuthandiza ine na m’bale George kumasulila mabuku ofotokoza Baibo m’citundu cacikulu ca ku Pakistan , cochedwa Ciudu . Pamene n’nabadwa , makolo anga anali kale ndi ana atatu , mkulu wanga mmodzi na azilongosi anga aŵili . Abale a ku Lusitara ndi ku Ikoniyo , mzinda umene uli pa mtunda wa makilomita 32 kucoka ku Lusitara , ‘ anamucitila umboni wabwino ’ Timoteyo . Ndiyeno , anapilila kwa zaka zambili m’ndende ku Iguputo pa mlandu umene sanacite . Mwina mungakhumudwe n’kuyamba kuona ngati kutumikila Yehova n’kosakondweletsa . Pemphani Yehova kuti akuthandizeni kuzindikila mmene onse m’banja akumvelela . 6 : 14 - 16 , 22 ; 2 Pet . ( Chivumbulutso 19 : 11 - 13 ) Yesu Khristu ndiye amachedwa Mau , cifukwa ni wokambilako Mulungu . Kukhala ndi wina amene ayang’anila makolo okalamba , kungacepetse nkhawa zimene anawo angakhale nazo . Kodi Amalonda Amene Anali Kugulitsa Ziweto M’kacisi Anali “ Acifwamba ” ? Paulo anapeza kuti mnyamatayu wapita patsogolo kwambili kucokela paulendo wake wapita . 19 : 29 . Motsogoledwa ndi Mfumu yathu , anthu a Mulungu agwilitsila nchito njila zosiyanasiyana kuti afikile anthu ambili polalikila . Choong Keon anati : “ Tinali kugwila nchito ya maola ocepa , ndipo tinali kukhala bwino kwambili . ‘ Pitilizani Kulimbikitsana Tsiku na Tsiku , ’ Nov . Ngati n’conco , mufunika kusankha mabwenzi amene atumikila Yehova kwa nthawi yaitali ndipo amalimbikitsa mgwilizano mumpingo . Upita ku ndende yozunzilako anthu , ndipo ena onse apita ku Siberia . N’zoona , Yehova sagwilitsa mwala anthu amene amamutumikila mwakhama . Kodi Nkhondo ya Aramagedo N’ciani ? M’bale William , mkulu wodalilika amene watumikila kwa zaka zoposa 20 , anapeleka malangizo kwa amuna oikidwa catsopano pa udindo . Anati : “ Muzikonda abale . Carin , mwamuna wake ndi ana ao ndi osangalala kwambili kuti anasankha kuti azikhala pamodzi . Timadziŵa bwanji kuti fanizoli limagogomezela nchito yolalikila ? Kodi mkwatibwi ameneyo wakonzekeletsedwa bwanji kaamba ka cikwati ? Akristu oona anatengela citsanzo cake mwa kulalikila “ uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu ” kulikonse . Mu 1961 , akatswili ofukula zinthu zakale anapeza mwala umene panali dzina la Pilato m’Cilatini pamene anali kufukula zinthu zakale m’bwalo la maseŵela la Aroma limene linali m’dela la Kaisareya , ku Israel . Tifunika kudziŵa kuti n’zotheka kutaya cikhulupililo cathu . ( Yesaya 40 : 22 ; 55 : 8 , 9 ) Conco n’zosadabwitsa kuti pali mfundo zina zokhudza Mulungu zimene anthufe sitingathe kuzimvetsa . Kodi tiyenela kucita ciani ngati talakwitsa zinazake n’kulephela kucilikiza ulamulilo wa Mulungu ? Pa ubatizo wa Yesu , Yohane Mbatizi anaona “ kumwamba kukutseguka , ndiponso mzimu ukutsika ngati nkhunda kudzamutela . ” ( b ) N’ciani cimene anamwali anzelu anatanthauza pamene anauza anamwali opusa kuti apite kukagula mafuta ao ? Anthu ambili m’dzikoli amaika maganizo awo onse pa kukhutilitsa zilakolako za thupi . Iwo anapemphela kwa Mulungu osati kwa Yesu . Tinapita patsogolo mwamsanga , cakuti tinatsiliza kuphunzila buku lophunzilila m’miyezi iŵili cabe . N’ciani cingatithandize kukhalabe paulendo wathu wopita ku cipulumutso ? Mdani ameneyu ndi mtima wodzikonda . Iwo amaimila angelo amphamvu amene anawononga mzinda wa Yerusalemu , ndipo adzawononganso dzikoli loipa la Satana pa Aramagedo . Tinalinso kusangalala ndi nchito yokonzekela misonkhano ikulu - ikulu . Otsatila a Kristu ocepa cabe ndi amene adzakhala ndi mwai umenewu . Apun Mambetsadykova Ndipo pamene tikali acinyamata amphamvu , timaganiza kuti mdani wathu ameneyu sangatifikile . Kuti mupindule ndi kuŵelenga Baibo , khalani na colinga cofuna kudziŵa cinacake cimene cingakuthandizeni pa umoyo . Tisamagwile nchito mwakhama ndi colinga cakuti tikhale ndi umoyo wapamwamba kapena kuti tipeze ndalama zodzagwilitsila nchito mtsogolo . N’ciani cimene Akristu amene ali pa cisumbali ayenela kuphunzila pa kukhulupilika kwa Msulami ? Mariya anali ndi cikhulupililo capadela kwambili . Musalole zimenezo kukukhumudwitsani . 8 : 28 - 32 ; Maliko 5 : 1 - 5 ) Sitiyenela kudelela mphamvu za ziwanda kapena za “ wolamulila ziwanda . ” ( Mat . Malangizo amenewo anam’thandiza kuyambanso kuona zinthu moyenela . Si paja iwo anali ndi cakudya ca mwana alilenji . 9 , 10 . ( a ) Satana anamuneneza ciani Yehova ? Anatiuza kupita ku matauni a kum’mwela ca kum’mawa kwa England . Timayamba kukonda kwambili abale athu . Kodi banja lina linakamba ciani za umoyo wao mu utumiki wanthawi zonse ? Fufuzani Bwinobwino . “ N’ciani cinatithandiza kupilila ? Ngakhale kuti maiko ambili ndi olemela , anthu oculuka ali mu umphawi wadzaoneni . Ngakhale kuti tili na mbali zosiyana - siyana , tonse ndife ofunika . ( Yohane 8 : 32 ) Masiku anonso , coonadi cimene Yesu anaphunzitsa cikumasula anthu m’njila zambili . — Onani bokosi yakuti “ Kumasuka mu Ukapolo wa Mtundu Wina . ” ( Zek . Ndi zocitika ziti zofanana ndi za mu 66 C.E . zimene zidzacitika posacedwapa ? 10 : 32 , 33 . Pa Aheberi 12 : 2 pamati : “ Cifukwa ca cimwemwe cimene anamuikila patsogolo pake , anapilila mtengo wozunzikilapo . Iye sanasamale kuti zocititsa manyazi zimucitikila , ndipo tsopano wakhala pansi kudzanja lamanja la mpando wacifumu wa Mulungu . ” Tinali kufika panyumba tili olema , koma tinali acimwemwe . ” Ni maganizo anji amene amakopa anthu ambili ? 4 : 5 - 20 ) Naise masiku ano , tatsimikiza mtima kupitilizabe kukonda Khristu , kuona moyenela nchito yakuthupi , zosangulutsa , na cuma . Nanga zimenezi zimakupangitsani kumva bwanji ? Iye anatonthoza ophunzilawo . Tingapezele bwanji banja lathu zinthu zofunika popanda kupita ku dela lina ? Koma ngati timangoganizila zolakwa zathu zakale , tingayambe kukaikila kuti Yehova anatikhululukila macimo athu . 3 : 23 , 24 ) Cilamulo citafafanizidwa pa imfa ya Yesu , Mulungu anakhazikitsa makonzedwe atsopano . ( Aheb . 3 : 14 , 15 . Tiyelekeze kuti wa Mboni , dzina lake ndi M’bale Mumba , afika pakhomo la a Daka . Titapita patsogolo kwambili ndi nchito yovina , tinaganiza zoleka nchitoyo . ( Genesis 21 : 6 ) Mphatso ya Yehova yozizwitsa imeneyi inam’sangalatsa masiku ake onse . kusiyana kwa cuma cakuthupi ndi cuma ca kuuzimu ? Kucokela pa nthawi yoyendelana , cikondi cawo cakula mpaka kufika polumbila kuti adzakhulupilika kwa wina ndi mnzake m’cikwati . 22 . KOSONGOLELA pensulo kooneka monga boti m’manja mwa Jordan , kanali kuoneka kacabe - cabe . Koma kudziŵa cabe tanthauzo la zizindikilo zimenezi , pakokha si kokwanila . Onse amene anali kugwilizana ndi Yesu anafunika kusintha zinthu zina paumoyo wao wa tsiku ndi tsiku . Kodi tingagwilitsile nchito bwanji Baibulo kuti tione ngati tili ndi mtima wodzikonda ? NYIMBO : 6 , 24 Zimene Yesu anauza mmodzi wa ocita zoipa amene anapacikidwa pamodzi naye , zingatithandize kupeza yankho . 12 : 10 . Mukanakhala kuti ndinu wophunzila wa Yesu ndipo mwadziŵa zimene Petulo wacita , kodi sembe munapitiliza kukhulupilila Yehova ? ( Yes . 55 : 8 , 9 ) Iye amafufuza atumiki ake ndi colinga cakuti aone makhalidwe ao abwino ndi kuwathandiza osati kuti awapeze zifukwa . Iye anati : “ N’nazindikila kuti ngati wacicepele ali na khalidwe lokonda zokopana adzakhala ndi mavuto akadzaloŵa m’banja . Ciyeso cimodzi covuta kwambili cimene makolo ena akumana naco n’cokhudza kuyanjana na mwana wocotsedwa . Cidziŵitso cimeneco cidzakhala maziko olimba a cikhulupililo ceni - ceni . Onani kuti sakucotsa mtendele m’maiko ocepa cabe , koma padziko lonse . Banja la Antoine linadziŵa za Ophunzila Baibulo kudzela mwa amalume ake amene anapezeka koyamba ku msonkhano mu 1924 . 4 : 11 . Timacita kusankha tokha . Ndithudi , sitiyenela kunyalanyaza mwai wapadela kwambili umenewu . — Ŵelengani Salimo 145 : 14 - 16 . Ofesi ya nthambi kapena akulu mumpingo alibe mphamvu yosankhila Mkristu cithandizo ca mankhwala , ngakhale kuti iye wafunsila kwa io . Pontiyo Pilato anafunsa Yesu kuti : “ Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda ? ” Mtimawo umaphatikizapo zimene munthu amalaka - laka , maganizo ake , makhalidwe , maluso , ndi zolinga zake . Zipatso za mtengo wamkuyu Fotokozani citsanzo cimene cionetsa kuti kuceleza sikulila kukhala na zinthu zambili . Kaŵili - kaŵili , kumwetulila mwaubwenzi kumakhala ciyambi cabwino ca makambilano . Kagulu kocepa ka anthu okhulupilika kocedwa “ kagulu ka nkhosa ” n’kamene kanasankhidwa ndi Mulungu kuti kapite kumwamba . Conco , kumvela Mulungu kumatanthauza kuphunzila na kutsatila zimene iye amakamba . Iwo anali kudziŵa kuti Mulungu anathandiza mneneli Eliya ndi Elisa kucita zozizwitsa zimenezo . ( 1 Maf . ( Ezekieli 37 : 2 , 11 ) Zimenezi zikuonetsa kuti anthuwo anali akufa kwa nthawi yaitali . Pocita maseŵelawo , tinali kukambilana ndi ana athu . 20 : 9 , 10 ) Nanga bwanji za lonjezo lakuti m’tsogolo akufa adzauka , mwina pambuyo pa zaka zambili ? Ngati mwacita zimenezi , mosakaika ‘ mudzalaŵa ndi kuona kuti Yehova ndi wabwino . ’ — Sal . Tili mu ulaliki na adzukulu athu Zopeleka zimenezi amaziseŵenzetsa popititsa patsogolo nchito yolalikila padziko lonse . Izi ziphatikizapo kucilikiza amishonale na atumiki a nthawi zonse apadela . ( Mac . Conco , kuti ophunzilawo akhale ogwilizana , anafunika kusintha mmene anali kuonela zinthu . 30 : 20 , 21 ) Popeza kuti tinadzipeleka kwa Yehova , iye amafuna kuti azititsogolela ndi kutiteteza kuti tisavulale mwakuuzimu . ( Ŵelengani 1 Timoteyo 1 : 12 - 14 . ) Kodi n’zocitika zanji zimene zinapangitsa kuti akhale m’nyumba imodzi usiku wonse ? 32 : 2 ) Zimenezi ndi zolimbikitsa kwambili . ( Ŵelengani Yeremiya 17 : 9 , 10 . ) Pamene muŵelenga za masomphenya amenewa , kumbukilani kuti kumwamba kumene tikamba pano ni malo auzimu , amene kulibe zinthu zooneka kapena zogwilika . Kodi Akhristu oona analoŵa liti ukapolo kwa Babulo wamkulu ? ( 2 Timoteyo 3 : 16 ) Baibulo limatithandiza kudziŵa zambili zokhudza Mlengi komanso kuti tikhale ndi umoyo wabwino . M’bale Erlenmeyer anali ndi zaka pafupifupi 10 zakubadwa pamene anagwilitsila nchito khadi la ulaliki kwa nthawi yoyamba . Makolo amafunika kulankhulana momasuka ndi ana ao kuti azikondana ndi kukhulupililana . ( Mlal . 9 : 2 , 10 ) Ngati ndinu wacinyamata ndipo mumaganizila kwambili za colinga ca moyo wanu ndi utali wake , kodi si canzelu kupewa ‘ kuyenda monga mmene anthu a mitundu ’ amayendela ? Mukamayesetsa kucita zimenezo , mudzakhala ndi moyo watanthauzo . — Aef . Panthawi imodzimodzi timalemekeza kwambili udindo umene Yesu ali nao pa kutithandiza kuti tikapulumuke . 1 , 2 . ( a ) N’ciani cionetsa kuti vuto la kusagwilizana m’dziko likukulila - kulila ? Mogwilizana ndi ulosi umene Mulungu ananena wa pa Genesis 3 : 15 , Satana mosakaikila anali kufuna - funa mpata woukila Aisiraeli amene anali kuoneka kuti alibe thandizo . 21 Kodi Baibulo Likusinthabe Umoyo Wanu ? 3 : 1 , 13 ) Koma tisalole zimenezi kutilepheletsa kukhala acifundo kapena kutilanda cimwemwe cathu . Koma panapelewela mpeni umodzi kuti akwanitse kucita zimenezi . Koma sizingakhale conco iyai . Pemphelo limanithandiza kupilila cifukwa Mulungu nimam’khulupilila komanso nimadziŵa kuti amanikonda . ” Kodi anthu a Yehova a m’nthawi yakale anapeleka bwanji citsanzo cabwino pa nkhani yocita zopeleka zothandizila ( a ) pa nchito zapadela ? Cifukwa ca kusakhulupilika kwa Solomo , Mulungu anali atakambilatu kuti ufumu wa Isiraeli udzagaŵikana . — 1 Maf . ( Yes . 52 : 9 , 10 ) Nthawi zonse muzikumbukila kuti mufunika kupitilizabe kukhala m’gulu la anthu a Mulungu kuti mudzapulumuke . Ganizilani citsanzo ici : Mukafuna kupita kumalo amene simunapiteko , mumayamba mwafunsa munthu kuti akuuzeni njila ndi zizindikilo zimene zingakuthandizeni kuzindikila malowo . Ndithudi , kuonetsa cidwi kwa alendo kumathandiza kuti maceza akhale okondweletsa . “ Odala ndi anthu acifundo , cifukwa adzacitilidwa cifundo . ” kudziŵa colinga ca Yehova na cifunilo cake kumatithandiza kukhala acimwemwe . PA CIKUTO : Akugaŵila magazini a Galamukani ! Kodi lemba la Maliko 5 : 25 - 34 limaonetsa bwanji kuti Yesu anali kucitila cifundo odwala ? Tinakusowani . ’ ” Ngakhale kuti abale akewo anamucitila nkhanza , iye sanawakhaulitse koma anawayesa kuti aone ngati anasinthadi . Mphatso zina ni za mtengo wapatali cifukwa zimakwanilitsa zosoŵa zathu , ngakhale zofunika kwambili . Imeneyi ndi nchito yaikulu . ( Salimo 139 : 16 , 23 ) Conco , Davide anali wotsimikiza kuti ngakhale kuti anacimwa , ndipo nthawi zina anacita macimo aakulu , Yehova anaona kuti anali ndi mtima wolapa . ( Yoh . 3 : 16 ) Pali anthu ambili amene anakhalako pa ubwenzi wolimba ndi Yehova . Mulimonse mmene zingakhalile , dziŵani kuti pamene munali mkulu munali kuthandiza ena m’njila zambili . Komabe , akazi ambili amene ali ndi cuma cambili amakhalabe ovutika maganizo ndi amantha . Anthu ambili a ku Ulaya anavutika ndi njala pamene nkhondo inatha mu 1918 . Sukulu n’nalekeza giledi 5 , ndipo n’nayamba kuseŵenza pa famu . 10 : 19 . Kodi ndinu wolimba mtima cakuti mungavomeleze kuti Yesu ndiye Mfumu yanu ? Moti iye anadzifunsa kuti , kodi mnyamata ameneyu angakhale kuti amalankhula ndi Yehova ? — Genesis 37 : 6 , 8 , 10 , 11 . 45 : 3 , 5 ) Kodi muganiza n’ciani cikanacititsa Baruki kukhala wacimwemwe ? Titadya cakudya ca m’maŵa , mwacizoloŵezi tinapsompsonana , tinakumbatilana ndipo tinauzana mau akuti ‘ Ndimakukonda , ’ kenako iye anapita ku nchito . Kucita zimenezi kudzaonetsa kuti cikhulupililo cathu n’colimba . — 1 Atesalonika 5 : 17 . Iye anapemphela mocokela pansi pamtima kuti : “ Inu Yehova mukafuna kuthandiza , zilibe kanthu kuti anthuwo ndi ambili kapena ndi opanda mphamvu . Amakonda kwambili ciwelewele , ciwawa , ndi ndalama . Patapita pafupifupi mwezi umodzi ataloŵa m’Cipululu ca Sinai , cakudya cao cinayamba kucepa . 18 “ Munthu Wopatsa Mowolowa Manja Adzalandila Mphoto ” Kusinkhasinkha kumatanthauza kuika maganizo pa cinthu cinacake , kuciganizila mozama ndiponso mosamala kwambili . Afunika kuonetsa makhalidwe amene mzimu woyela umatulutsa ndi kukwanilitsa ziyeneletso za m’Malemba . 9 : 3 - 5 , 15 ; 22 : 6 - 8 ) Komanso , ganizilani mapindu oculuka amene tingapeze ngati tiŵelenga mabuku a m’Baibo amene Yehova anauzila Paulo kulemba . Zimene anthu amafuna zimasiyana kwambili malinga ndi dela limene amakhala . 1 : 14 ) Inde , Timoteyo anafunika kudalila mzimu wa Mulungu kuti apilile pocita utumiki wake na kuti aziukonda . Kenako iye anafotokoza mmene kuphunzila Baibo kunamuthandizila kusintha . Kodi vuto limene mwina linabuka cifukwa ca kusiyana zinenelo mumpingo wacikhristu linathetsedwa bwanji ? Tinagaŵila tumabuku topitilila pa 20,000 , ndipo maina a anthu ofuna kuphunzila coonadi tinawatumiza ku ofesi ya nthambi ya Britain . Ndi zinthu zotani zimene Abulahamu , Isaki , ndi Yakobo ‘ anaona ’ ? ( Yoh . 7 : 47 - 49 ) Iwo anali kuona kuti aliyense amene sanaphunzileko ku sukulu ya Arabi , kapena amene sanali kusunga miyambo yawo , ndi munthu wamba wosanunkha kanthu . ( Mac . N’ciani cinathandiza Mose kutsogolela Aisiraeli ? Mngelo wacisanu ataliza lipenga , Yohane anaona “ nyenyezi imene inagwela kudziko lapansi kucokela kumwamba . ” amakuphunzitsilani coonadi ? ( 1 Akor . 14 : 31 ) Cristina , amene tamutomola kuciyambi kwa nkhani ino anati : “ Cimene nimakonda kwambili ku misonkhano ni cikondi na cilimbikitso cimene nimalandila kumeneko . Onani mau ocokela m’Baibulo , ndi kuganizila mayankho amene apelekedwa . Kenako , onse a 144,000 pamodzi na Yesu adzamenya nkhondo yogonjetsa mafumu onse a padziko lapansi . 4 : 4 ) Conco , ni mwayi wathu kutengela citsanzo ca Yesu mwa kuthandiza anthu kudziŵa Yehova , Mulungu waufulu , na kuyamba kumulambila . ( Mat . Kunena zoona , Yehova amakondwela kwambili ndi mzimu wogwilizana umenewu . TSAMBA 7 M’zaka zaposacedwapa , Utumiki Wathu wa Ufumu wakhala ukulimbikitsa abale ndi alongo kuti aziganizila ena pankhani yogwilitsila nchito pelefyumu akamabwela ku misonkhano yacigawo . Iye sangakondwele ngati tiyesa kudzipulumutsa tekha ndi “ mphamvu za hatchi , ” kapena kuti kudalila zinthu zimene anthu a m’dzikoli amadalila . Sakanathanso kulewa zotulukapo za macimo ake . N’cifukwa cake mungafunse kuti : ‘ Kodi cikondi cimakhalitsadi ? Iye angatithandizenso kulamulila maganizo athu opanda ungwilo . — Sal . Izi n’zosadabwitsa kwa anthu amene amaphunzila Mau a Mulungu , cifukwa Baibo inakambilatu kuti cimodzi mwa zizindikilo za “ masiku otsiliza ” n’cakuti anthu adzakhala “ osadziletsa . ” — 2 Tim . Yehova anasinthilatu umoyo wanga . Ku Frankfurt , m’dziko la Germany m’caka ca 1951 , abale akhama anacita lendi makina ena ake ndi kuwagwilitsa nchito kutenthetsa maketulo 40 ophikila . Pambuyo pothila mafuta m’motoka yathu , n’napempha kwa wanchito wa pamenepo kuti mkazi wanga aseŵenzetseko toileti ya pa malowo . Thandizani ana anu kukonda utumiki ( Onani ndime 11 ) 1 : 31 ) Inde , “ zonse ” zimene Yehova anapanga zinali “ zabwino kwambili . ” Ndinalibe cidalilo cakuti ndingakhalenso wodalilika . ( 2 Mbiri 11 : 5 - 12 ) Cofunika kwambili cinali cakuti , kwa kanthawi anamvela malamulo a Yehova . Koma Yehova na Yesu amakondwela kwambili na mgwilizano umenewu . Kuti iye akhale “ mwala wofunika kwambili wapakona , ” anaukitsidwa . — w17.12 , mape . Ngati oweluza ndi ozindikila , osakondela ndi opanda ziphuphu , anthu amathandizidwa . Iye anakhalabe wokhulupilika kwa Mulungu . ( Maliko 6 : 3 ) Conco , ayenela kuti anali wamphamvu . Komanso kungasokoneze mtendele mumpingo . ( Aef . Anthu a Mulungu akakumana pamodzi kuti aphunzitsidwe amasangalalanso kwambili kudya cakudya cakuthupi pamodzi . Anapemphela kwa Yehova . Inde , cimwemwe coculuka cimene timapeza , cimatipatsa mphamvu yopitiliza kulalikila ngakhale m’magawo ouma . — Mat . Monga kholo , muli na udindo waukulu ndiponso mwayi wolela ana anu “ m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake . ” ( Aef . Koma m’nthawi ya Sara , sitima za amalonda zinali kuyenda - yenda mumtsinje wa Firate , kubweletsa katundu wamtengo wapatali mumzinda wolemelawu kucokela m’madela akutali . Maluwawo afota . Koma mau a Mulungu wathu adzakhala mpaka kalekale . ” — YES . Pambuyo pofufuza zeni - zeni zimene zinacitika , bungwe la akulu lidzaona ngati anthuwo ni ofunika kuwapangila komiti yaciweluzo kapena ayi . Wodala ndi munthu amene Yehova sanamusungile colakwa cake , amene alibe mtima wacinyengo . ” ( Yos . 24 : 15 ) Sitingakuuzeni kuti mukwatile kapena ai , sitingakusankhileni munthu amene mungakwatilane naye , kapena nchito imene muyenela kugwila . M’cinenelo ca Cikabeka NYIMBO : 45 , 36 Timalemekeza zikumbumtima za ena , ndiponso timafuna kukhala zitsanzo zabwino . Yesu atatsala pang’ono kuphedwa , anacenjeza ophunzila ake katatu za “ wolamulila wa dzikoli . ” Yesu mu ulemelelo wake anaonekela kwa mtumwi Yohane m’masomphenya ndi kukamba kuti : “ Wopambana pa nkhondo ndidzamulola kukhala nane pampando wanga wacifumu , monga mmene ine ndinakhalila ndi Atate wanga pampando wao wacifumu . ” ( Chiv . Akristu odzozedwa amene adzaonetsa ‘ kukhulupilika kwao mpaka imfa adzapatsidwa mphoto ya moyo kumwamba ’ . N’zotheka kukhalabe okhulupilika . M’maiko ambili , Mabaibulo ndi odula kwambili ndipo ndi ovuta kupeza . Yesu anakamba kuti iye ali monga m’busa , ndipo otsatila ake ali ngati gulu la nkhosa . Tikatelo , tidzapeza thandizo limene tifunikila kuti tilimbitse cikhulupililo cathu . ( b ) Kodi kusiyana kumene kulipo pakati pa Yesu na Herode Agiripa Woyamba kutiuza ciani ponena za mtsogoleli amene Yehova amasankha ? Robert akupitiliza kuti : “ Cinthu cofunika kwambili paumoyo wathu tsopano ndi kugwila nchito zampingo . Amuna ndi akazi , okalamba ndi acicepele , ngakhalenso ana , anali kumasuka naye . Iye anacitanso zozizwitsa zina zambili . Mkati mwa ulendowo , Olipa anasankha kubwelela kwao ku Mowabu . Kali ndi mafunso okwana 6 amene anthu amafunsa . Koma m’kupita kwa nthawi , Aisiraeli anaumitsa mitima yawo ndi kutaya cikhulupililo cawo . Conco , ambili analephela kuloŵa mu mpumulo umenewo . ( Num . 14 : 30 ; Yos . Kukamba zoona , Yehova sananisiyepo . N’nali kucita zinthu mopanda ulemu . 5 : 29 ) Mouzilidwa , Lameki anati : “ Uyu ndi amene adzatibweletsele mpumulo ku nchito yathu yopweteketsa manja , cifukwa colima nthaka imene Yehova anaitembelela . ” Nanga n’cifukwa ciani safunika kucita mantha ? Izi n’zimene ninacita , ndipo zinanipindulitsa kwambili ! David : Nditamvetsetsa kukwanilitsidwa kocititsa cidwi kwa maulosi a m’Baibulo , monga ulosi wa pa Mateyu 24 ndi wa m’buku la Danieli , ndinatsimikiza mtima kuti ici ndico coonadi . Kapena acibale osakhulupilila a Mkhristu angayambe kumukakamiza kuti akwatile kapena kukwatiwa kuti ‘ angakalambile pamphala . ’ Masiku ano , mabuku ambili , mafilimu , na mapulogilamu a pa TV , amalimbikitsa ana kukhala osamvela makolo kapena kuona ngati khalidweli lilibe vuto . Koma zoona zake n’zakuti kusamvela makolo kumasokoneza mtendele wa banja , lomwe ndilo maziko ofunika a cikhalidwe ca anthu . ( Mateyu 24 : 14 ) Uthenga wabwino ukalalikidwa mokwanila , Ufumu wa Mulungu udzabwela kudzaononga dziko loipali . Mpingo woyamba m’dela limeneli utakula , anaugaŵa . Njila yofunika kwambili yoonetsa kukhulupilika kwathu kwa Mulungu ni kutsatila malangizo a gulu lake . Inakamba kuti padziko lapansi palibe phili lalitali lakuti munthu angaimililepo n’kuyamba kuona maufumu onse a dziko lapansi . Kuona mtima kotele kumapezeka kokha pakati pa anthu amene amatumikila Mulungu mopanda cinyengo . Iwo anadzimva monga mmene anamvelela Rute , mkazi wacimowabu , amene anauza Naomi , mkazi waciisiraeli , kuti : “ Anthu a mtundu wanu adzakhala anthu a mtundu wanga , ndipo Mulungu wanu adzakhala Mulungu wanga . ” Kodi Yesu anauza ophunzila ake kuti aziyembekeza anthu kubwela kwa io ? Pamene anakula , tinayamba kuganizila zokatumikila ku dziko lina . ” Conco , pemphani Yehova ‘ kuti cikhulupililo canu cisathe . ’ “ Tionjezeleni Cikhulupililo ” Kodi Baibulo ndi Locokela kwa Mulungu ? Yehosafati ndi Ahaziya anali kumangila pamodzi zombo . N’ciani cingatithandize kuti tizikonda kwambili coonadi ? Amayi anali munthu wokonda kupemphela . Mtumwi Paulo pamenepa sanali kufotokoza za mzela wobadwila wa Mesiya . Masheya : Mungapeleke ku gulu la Mboni za Yehova masheya amene muli nawo m’kampani kapena mungakonze zakuti lidzalandile masheyawo mukadzamwalila . 10 , 11 . ( a ) Ndi zinthu ziti zimene zingayese cikhulupililo cathu ? Pamene tikambilana zitsanzo zimenezi , onani mmene zingakuthandizileni kuikabe maganizo anu pa zinthu zauzimu ndi kuteteza ubwenzi wanu ndi Yehova , maka - maka pamene muona kuti ena akucitilani zinthu zopanda cilungamo . Kunali kupanduka ndi kusayamikila zinthu zabwino zimene Yehova anamupatsa . ( 1 Tim . 4 : 8 ) Zoona , kukhala na cidalilo colimba cakuti Yehova “ amapeleka mphoto kwa anthu omufuna - funa ndi mtima wonse , ” kudzatithandiza kukhala olimba m’cikhulupililo . — Aheb . Masiku ano , anthu acifundo ngati Msamariya uja sapezekapezeka . Wamasalimo anaimbila Yehova kuti : “ Mudzanditsogolela ndi malangizo anu . ” Mu 1911 , paulendo wa namba 6 na 7 wa M’bale Russell , nkhani za poyela zimene zinalengezedwa zija nazonso zinakambidwa . Pambuyo pake , Milton analembanso ndakatulo ina yakuti Paradise Regained ( Paradaiso Wobwezeletsedwa ) . Kodi ndimaleka kukambitsana naye ? 7 : 39 ) Kodi mumamvela bwanji akulu akapeleka nkhani yacenjezo ? ( Maliko 6 : 30 - 32 ) Kukambilana mwa njila imeneyi kunacititsa Yesu ndi atumwi ake kukhala paubwenzi wolimba . Kunacititsanso atumwi ake kukhala okonzeka kugwila nchito imene anali kudzacita mtsogolo . Baibo imaonetsa kuti , kuyambila kale , anthu a Mulungu akhala akucita zopeleka . Ngati tiyenela kuonetsa Khalidwe Lopambana kwa adani athu , bwanji ponena za anthu amene timalalikila , anthu amene ali ndi ‘ maganizo abwino amene angawathandize kukapeza moyo wosatha . ’ — Mac . 13 : 48 . 28 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi ( 1 Mafumu 17 : 17 - 24 ; 2 Mafumu 4 : 17 - 20 , 32 - 35 ) Masiku ano , anthu odwala amafunanso kudziŵa ngati Mulungu adzacitapo kanthu kuti awacilitse . Mngeloyo anacitanso cidwi ndi cinthu cina . Popeza tili ndi cikhulupililo colimba m’malonjezo a Yehova , tiyeni tikonzekele kudzakhala m’dziko latsopano . Umu ndi mmene zinalili ndi mphatso imene a Russell , amene tawachula kuciyambi kwa nkhani yapita , anapatsa Jordan . Colinga cake cacikulu ndi kutsogolela nkhosa ku “ msipu wabwino . ” ( Ezek . Nili ku sukulu ya apainiya ya cinenelo camanja ca ku America . Nthawiyi n’nali na zaka 79 ( Lev . 8 : 4 , 5 ) Mofananamo , nthawi zonse tizicita zimene Wolamulila wathu , Yehova , amafuna kuti ticite . Koma coyamba , tiyeni tikambilane umboni wa pa Yesaya 40 : 26 - 31 , woonetsa kuti Yehova angakwanitse kutipatsa mphamvu zopilila mavuto . Kodi Sukulu ya Gileadi yakhala yothandiza ? N’cozizwitsa citi cimene cinacitika pa Pentekosite wa mu 33 C.E . ? Kodi mapemphelo ndi mapembedzelo opelekedwela mu tuakacisi amayankhidwa ? Apainiya anthawi zonse amapeleka maola 70 a mu ulaliki pamwezi . Ine na mkazi wanga timaukonda umoyo wa pa Beteli . N’cifukwa ciani tidzafunika kukhala ogwilizana kwambili panthawiyo ? Kodi inu mumakaika ngati mungakwanitse kukatumikila monga mpainiya ku dziko lacilendo ? M’zikhalidwe zina , alendo amene sanaitanidwe amalandilidwa . Ngati pali nchito ina iliyonse imene mufunika kugwila , igwileni mwamsanga . ” — Christian . Ndipo pamene tikucita zimenezi tiyenela kukhulupilila kuti Yehova adzatithandiza kulimbana ndi mavuto amene tikukumana nao tsopano , ndiponso amene tingakumane nao mtsogolo . Mu 1989 , mpanda wochedwa Berlin Wall unagwetsedwa , ndipo Cikomyunizimu m’cigawo ca kum’maŵa kwa Ulaya cinathela pomwepo . Maganizo oipa komanso cilako - lako coipa zinam’sonkhezela kucita chimo . Kuti tikhulupilile kuti Yehova amatikonda , coyamba tiyenela kukhulupilila kuti iye ndiye anatipanga ndi kutipatsa moyo . 12 : 12 ) Kucokela nthawiyo , io akhala akulalikila ‘ m’masiku otsiliza ’ ano omwe ndi “ nthawi yapadela komanso yovuta . ” — 2 Tim . Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 , tsamba 28 , ndime 8 - 10 inafotokoza yemwe ali kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . Ndipo tidzapitiliza kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu mpaka pamene mapeto adzafika . Mwamuna mmodzi akuchulidwa kuti “ wocenjela . ” Munda wochingidwa sumakhala woonekela kwa anthu onse . Amacita zimenezi cifukwa amafuna kutiteteza monga mmene anali kucitila kwa Aisiraeli . Amandifunsa mafunso anzelu ndipo zimenezi zandithandiza kuwafotokozela nkhawa zanga . Cifukwa cakuti cikhulupililo ndi limodzi mwa makhalidwe amene mzimu woyela umatulutsa . M’bale Jürgen Rundel ndiye anali kutsogolela pa nchitoyi , ndipo anali kuigwila m’njila zosiyanasiyana . Anayamba kulalikila anthu aciabolijini ndi kukhazikitsa mipingo yatsopano . M’baleyu anadziŵika kwambili ndipo anthu anali kum’lemekeza kumadela onse akutali . Cifukwa ca kunyada , apandu amenewo anadzipangila makonzedwe ao olambilila Yehova . 3 : 12 ) Kukamba zoona , kupemphela kwa Yehova ni njila yaikulu kwambili imene waonetsela kukoma mtima kwakukulu . Iwo amakhala pafupi na sitesheni ya basi n’kumagaŵila mabuku ofotokoza Baibo kwa anthu opita pamalowa . Tiyelekezele conco : Mwana dzina lake Johnny akuseŵeletsa bola m’nyumba . A Yohane : Ndine Yohane . Conco , ndinaona kuti panalibe condiletsa kuyamba upainiya . Ndiponso pamene tikulalikila ena , timawafika pa mtima . 13 : 24 - 30 , 36 - 43 ) Onani Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 , tsamba 15 - 18 . Kuonjezela apo , ubweya anali kuupaka penti . Yehova watiphunzitsa coonadi cimeneci cifukwa amatikonda . ( b ) Kodi tiphunzilapo ciani tikaona mmene Abulahamu anathetsela mkangano ? N’cifukwa ciani n’zotheka kukhala paubwenzi ndi Yehova ? * Conco , nyengoyi iyenela kukhala nthawi yaitali kwambili . Nanga n’ciani cingacitike ngati alaliki akhama amenewa atacoka m’maikowa ? Mwina mulinso ndi mafunso ena . Iwo adzakuwononga limodzi ndi ana ako amene ali mwa iwe . Ndipo sadzasiya mwala pamwala unzake mwa iwe . ” — Luka 19 : 43 , 44 . Panthawiyi , mwanayo anakhutila ndi yankho losavuta limeneli . 12 , 13 . ( a ) Ndani anali pakati pa Aisiraeli pamene io anayambanso kulambila Yehova ? Komabe , zina mwa zizindikilozo zimaonekela mwa odwala ambili . Conco , kwa zaka zambili , Yehova anali cabe ndi alambili okhulupilika ocepa padziko lapansi , koma analibe gulu la “ anthu odziŵika ndi dzina lake . ” ( a ) Kodi ca kumapeto kwa ma 1800 , panacitika ciani cinathandiza anthu ena kuyamba kumvetsa coonadi ? Yehova atamuuza kuti adzoze Sauli , mneneliyo anamvela ndi mtima wonse cifukwa ca cikondi osati mokakamizika . Mwacitsanzo , tinene kuti tikugogoda pacitseko ca nyumba ya munthu . 3 : 18 ) Kodi izi zitanthauza kuti sitingaonetse cikondi mwa zokamba zathu ? Iyai . Zili ngati dyonkho cabe poyelekezela ndi zimene adzacite m’dziko latsopano la Mulungu . 2 : 16 ) Ngati muli ndi ana , kodi mungawathandize motani ? Koma Baibo imakamba kuti panthawi ina , pakati pawo “ panabuka mkangano woopsa . ” Kaya mabwenzi athu ni a mumpingo kapena ayi , ngati iwo salemekeza miyezo ya Yehova , m’kupita kwa nthawi angaticititse kuwononga ubwenzi wathu na Mulungu . Afarisi sanali kukhululukila ena cifukwa anali kuwaona ngati acabe - cabe . Koma ise Akhristu tifunika kukhululukila ena . PALI zinthu zocepa zimene timafunikila kuti tikhale na moyo . “ MTEMBO WOYENDA ! ” Yankho yomveka bwino - bwino ili pa Aroma 8 : 6 , yakuti : “ Kuika maganizo pa zinthu za mzimu kumabweletsa moyo ndi mtendele . ” Koma kodi muganiza kuti anthu amene ni osiyana kwambili zibadwa sangacitile zinthu pamodzi mwamtendele ? Pokamba ndi anthu a ku Atene wakale , Paulo anati : “ [ Mulungu ] wakhazikitsa tsiku limene akufuna kudzaweluza m’cilungamo dziko lapansi kumene kuli anthu , kudzela mwa munthu amene iye wamuika . Ndipo wapeleka citsimikizo kwa anthu onse mwa kumuukitsa kwa akufa . ” ( Mac . Mukacita conco , mudzapindula komanso mudzacititsa kuti akulu azikondwela na utumiki wawo . Kwa kanthawi ndithu , n’nali kukhala na cisumbali canga , dzina lake Tony . Kodi Yehova anamvela bwanji na zimene Mose anacita ? Pamene muyamba kupeleka thandizo muyenela kudziŵa bwino matenda a makolo anu . César amene amakhala ku Brazil , anali kawalala wa mfuti . Komanso , mwamuna akakhala tate , maudindo ake amawonjezeka cifukwa amafunika kusamalila onse aŵili , mayi ndi mwana . Kunena zoona ndife osangalala kwambili . ” Ngati mumatumikila Yehova ndi mtima wonse , monga mmene mkazi wamasiye anacitila , mungakhale ndi cidalilo cakuti muli “ m’cikhulupililo . ” “ COTSANI MOYO WANGA ” Nkhondo yoyamba itangotha , tsoka lina limene linali loopsa kuposa nkhondoyo linayamba . Iye anati : “ Akulu amene asamukila ku malo amenewa amapeleka thandizo lacindunji kwa abale a kumeneko payekhapayekha . 11 : 1 , 36 - 38 ; 1 Maf . Baibulo limakamba kuti Eliya analakalaka kufa . Koma kumbukilani zimene zinacitikila Petulo . “ Onani Dziko Lokoma ” — M’kabuku kameneka muli mapu na zithunzi za malo ochulidwa m’Baibo 5 Mungacite Ciani Kuti Kuŵelenga Baibo Kuzikukondweletsani ? Iwo anang’amba zovala zao ndi kulila mofuula kuti : “ Kalanga ine mwana wanga ! 14 : 6 - 10 ) Komabe , Paulo anakamba kuti “ lonjezo loloŵa mu mpumulo [ wa Mulungu ] lidakalipo . ” ( Aheb . Komanso anapatsa anthu mtima wofuna kukhala ndi moyo mpaka kale - kale . ” Irina * , mpainiya wanthawi zonse ku North America , anali wokwatiwa kwa mkulu mumpingo , koma mkuluyo anakhala wosakhulupilika cakuti anam’siya ndi ana . 5 : 19 ) Kwa iye , anthu a m’dzikoli ali ngati “ kadyonkho ” cabe . Yosefe anali kukomela mtima akaidi anzake ndi kuwacitila ulemu Banja la Betuele linadalitsa Rabeka wokondedwa wao . Ngakhale kuti acinyamatawo tsopano ali pamaudindo aakulu , afunika kupitilizabe kufunsila ndi kutapako nzelu kwa aciyambakale pofuna kupanga zosankha . Pamene anali kukamba ndi munthu woyamba Adamu m’munda wa Edeni , Yehova ayenela kuti anagwilitsila nchito Ciheberi . Pofotokoza maganizo ake pankhani ya ziphuphu za m’boma , mkulu wa dipatimenti ya boma yoona za kayendetsedwe ka ndalama m’dziko la Nicaragua anakamba kuti : “ Ngati nzika za dziko ndi za ziphuphu , akuluakulu a boma sangalephele kukhala a ziphuphu cifukwa naonso ndi anthu . ” Kodi Petulo analakwitsa ciani pamene anali ku Antiokeya wa ku Siriya ? 3 : 13 ) N’zomvetsa cisoni kuti olambila Yehova ena aleka kukhala maso . Patapita mawiki angapo , mlongoyo anapita kwa m’bale uja na kumufotokozela kuti kwa nthawi yaitali , iye wakhala akulimbana na vuto lalikulu kunyumba kwake . M’zaka zimenezo , abale ambili anali kudzimana zambili kuti akapezeke pa misonkhano imene inali kucitikila m’madela ocepa ku Mexico . Komabe , tifunika kuphunzila mmene tingaseŵenzetsele mwaluso lupanga limeneli poikila kumbuyo zikhulupililo zathu , kapena powongolela maganizo athu . ( 2 Akor . 10 : 4 , 5 ; 2 Tim . Conco pamenepa , Solomo anaphwanyanso lamulo la Mulungu loletsa kukwatila akazi a mitundu ina . — Deut . ( Aefeso 2 : 4 , 5 ) Popeza kuti Yesu ali ku dzanja la manja la Mulungu , posacedwa adzayamba kulamulila dziko lapansi ndipo adzapeleka madalitso osaneneka kwa anthu onse omvela . 1 : 23 ) Kodi mumasinkha - sinkha na kupemphela kuti mudziŵe mmene mungaseŵenzetsele zimene mumaphunzila ? Ndiye cilakolako cikatenga pakati , cimabala chimo . Ndi makonzedwe otani amene athandiza pa nchito yomasulila Baibulo ? Palibe cinthu cingalimbitse cikhulupililo cako kupambana kuŵelenga Mau a Mulungu . ( Ower . 11 : 30 - 34 ) Kodi zimenezi zinatanthauza ciani kwa mwanayo ? Akristu odzozedwa amamva ngati mmene Petulo anamvela pamene anati : “ Atamandike Mulungu amenenso ndi Atate wa Ambuye wathu Yesu Kristu , pakuti mwacifundo cake cacikulu , anatibeleka mwatsopano kuti tikhale ndi ciyembekezo ca moyo mwa kuukitsidwa kwa Yesu Kristu . Anatibeleka kuti tikhale ndi colowa cosawonongeka , cosadetsedwa ndiponso cosasuluka . Iye anali wosangalala cifukwa ca nkhani yabwino imene anafuna kuuza mbuye wake , yakuti Rabeka adzakhala mkazi wa Isaki . Conco , Yesu anauza atsogoleli aciyuda acinyengo a m’nthawi yake kuti : “ Ufumu wa Mulungu udzacotsedwa kwa inu n’kupelekedwa kwa mtundu wobala zipatso zake . ” 20,860,000 Ndiponso mokoma mtima , Mulungu anaongolela maganizo olakwika a Eliya akuti Aisiraeli onse analeka kutumikila Yehova . Timapeza anthu a makhalidwe otelo pakati pa abale ndi alongo athu akuuzimu cifukwa cakuti pa nthawi imene tinali kudzipeleka kwa Mulungu tinalonjeza kuti tidzatsatila malamulo ake . Anacotsanso ambuye ake aakazi , a Maaka , pa udindo wawo monga “ mayi wa mfumu , cifukwa anapanga fano lonyansa kwambili . ” ( 1 Maf . Monga taonela m’zitsanzo zapitazi , Mulungu angathe kutonthoza anthu amene akumana na mavuto osiyana - siyana . Mipukutuyo inali na dzina la Mulungu m’zilembo za Ciheberi , ndipo M’baleyo anatifotokozela kufunika kwa mipukutuyo . Ngati ticita zimenezi , tidzapeleka ulemelelo kwa Atate wathu wakumwamba , amene timaimila dzina lake . Mfumu yake ni Yesu . Kuseŵenzetsa ndalama mwanzelu Nchito yomanga ku Wallkill ndi ku Warwick idzatha posacedwapa . Conco , abale amene anaitanidwa kuthandiza panchito yomanga imeneyi amadziŵa kuti utumiki wao wa pa Beteli ndi wa kanthawi . 1 : 21 , 22 . Kodi muyenela kucita ciani ngati mwayamba kusiyana maganizo ndi a m’banja lanu cifukwa cotsatila Yesu ? Mtsikanayu anali wodekha ndi wodzicepetsa kwambili . Adani amenewa anali alembi ndi Afalitsi amene anali ophunzila kwambili ndi anzelu . Pamene Abulamu ( Abulahamu ) na mkazi wake Sarai ( Sara ) , anamvelela Mulungu ndi kusamukila ku Kanani , dzikolo linali lodzala na macitidwe onyoza cikwati . Tinalangizidwa kuti , tikangokhazikitsa phunzilo la Baibo m’buku ya Zimene Baibulo Ingatiphunzitse , timafunika kupatula mphindi zocepa tikatsiliza phunzilo lathu , kuti tizifotokozela wophunzilayo za gulu la Mulungu . Kodi zotulukapo zinali zotani ? Pamene Paulo na Sila anali kuimba nyimbo zotamanda Mulungu m’ndende , kunacitika zinthu zimene sanali kuyembekezela . Koma sanaiŵale zimene analonjeza Mulungu . A zamalaiti , mapulamba , mainjiniya , oyendetsa ndeke , madokota , na ena onse amadalila malamulo amenewo kuti agwile bwino nchito zawo . Ngakhale kuti anthu a m’fanizoli anapeza cumaco m’njila zosiyanasiyana , onse aŵili anazindikila kuti zimene anapezazo zinali zamtengo wapatali , ndipo onse anali ofunitsitsa kudzimana zinthu zina kuti apeze cumaco . M’malomwake , anali kuseŵenzetsa Malemba . ( Mat . M’bale winanso , dzina lake Evangelos Scouffas , anati : “ Zinali monga kuti cinthu cina cake camphamvu catinyamula tonse pamipando yathu . Cifukwa cacikulu cokhalila na zolinga zauzimu n’cakuti , timafuna kuonetsa kuti timamuyamikila Yehova kaamba ka cikondi cake , komanso cifukwa ca zimene amaticitila . Simungakhulupilile kuculuka kwa makoini a siliva amene nakhala ni kutenga . ” 39 : 10 , 12 . Kunyada , kukonda cuma , ndiponso ciwelewele ndi zida zimene Satana amagwilitsila nchito . Ndiyeno tinafunikila kuzoloŵela anthu atsopano , dziko latsopano , ndi kuphunzila cinenelo catsopano . Kodi ndani amene adzakhala ‘ m’magulu a nkhondo ’ amene adzatsatila Kristu ? Koma zaka pafupifupi 50 zapitazo , ku Middle East anthu anapeza mwala umene panali dzina limeneli . Amateteza maluŵa ake kuti asaonongeke ndi tudoyo ndi maudzu . Yesu nthawi zambili anali kugwila mau a m’Malemba Acihebeli . ( Aroma 2 : 14 , 15 ) Mwacitsanzo , ena amalemekeza na kukonda makolo awo . Atumiki anga adzasangalala , koma inuyo mudzacita manyazi . Makolo — Wetani Ana Anu Yesu akalibe kupeleka malangizo amenewa , anaphunzitsa ophunzila ake kuti popemphela , azipempha atate wawo wakumwamba kuti awapatse zinthu zakuthupi . Olo kuti anakulila m’banja la Mboni , iye anakamba kuti : “ Misonkhano ndi kulalikila zinali kunicititsa ulesi . ” N’cifukwa ciani m’pomveka kuti Yesu amachedwa “ cipatso coyambilila ” ? Amenewa ‘ ndi amene adzatuluka m’cisautso cacikulu , ndipo acapa mikanjo yao ndi kuiyeletsa m’magazi a Mwanawankhosa ’ cifukwa coonetsa cikhulupililo m’nsembe ya dipo ya Yesu . Popeza tinalibe nyumba yathuyathu , tikatsiliza kucezela mpingo tinali kukhalabe m’nyumba imodzimodziyo mpaka pa Mande . Ena anali kunibweletsela mphatso , monga sopo , mafuta na zinthu zina , kuphatikizapo maluŵa ndipo anali kuzisiya pakhomo . Monga tinaphunzilila m’nkhani yapita , Yesu anayankha kuti , “ lamulo lalikulu kwambili komanso loyamba ” ndi lakuti , “ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi maganizo ako onse . ” Ambili amene atumikila mumpingo wa cinenelo cina aona kuti kuphunzila Baibo nthawi zonse m’cinenelo “ cimene anabadwa naco , ” kumawapindulitsa . 18 : 36 ) Mwa ici , iwo anali kudedwa ndi kuzunzidwa na boma la Soviet Union . Ndipo sanali kucita mantha kukumana ndi masautso , n’colinga cakuti alalikila uthenga wabwino kwa ena . A dokota anamuuza kuti , kwa zaka ziŵili , safunika kuyendetsa motoka . Ngakhale n’telo , Baibulo limatiuza momveka bwino kuti mapeto n’ciani . Ndiyeno , amayamba kum’khulupilila ndi kuphunzila kwa iye . Mwacitsanzo , m’Cilamulo cimene Mulungu anapatsa Aisiraeli munali malamulo amene anali kuwateteza ku makhalidwe otayilila a mitundu yowazungulila . Paulendo wacisanu umene tauchula kuciyambi , M’bale Russell anayankhanso mafunso a otsutsa . Kupangitsa Cikwati Cacikhiristu Kukhala Cacimwemwe , Aug . 2 : 16 ) Ndipo masiku ano kuposa kale , kuli zinthu zosangalatsa zambili zimene zimakopa anthu ndi kuwalimbikitsa ‘ kukonda zinthu zosangalatsa . ’ 1 , 2 . ( a ) Tiyenela kucita ciani kuti tidzapulumuke ? ( 1 Pet . 1 : 15 , 16 ) Tiyenela kupewa kudetsedwa ndi cipembedzo conama kapena ndi ndale za m’dzikoli . 19 : 11 , 14 , 15 . Panyumba pathu tinali kugwilizana ndi kukondana , ndipo makolo anga anali kuniphunzitsa makhalidwe abwino . Mwacitsanzo , olo kuti cikumbumtima cake sicingamuvutitse , iye afunikanso kuganizila cikumbumtima ca ena . M’malo mokhala maso ndi kuyang’anila Mbuye wawo , iwo anagonja ku zofooka zathupi ndipo anagona . ( Aroma 13 : 12 , 13 ) Kuti tipambane pankhondo yolimbana ndi “ zinthu zapadziko , ” zimene ndi zilakolako zathupi , tifunikila kuika maganizo athu pa zinthu zakumwamba . Muzilalikila mwakhama monga “ oyang’anila abwino amene alandila kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . ” — 1 Pet . Mofanana ndi Eliya , onse olemba Baibulo anali ‘ anthu monga ife . ’ — Yak . Kodi Akristu ena mumpingo anathandiza bwanji mlongo wina pamene anali mtsikana ? ( Mat . 18 : 9 ) Masiku ano , Akristu amene amatsatila malangizo amenewa ndi mtima wonse , sazengeleza kucitapo kanthu pa zinthu zimene zingawavulaze mwa kuuzimu . 8 : 44 . Inoki anasankha kutengela cikhulupililo ca Abele . Komabe , kuganizila zinthu zoipa kungativulaze . Mouzilidwa , Paulo anawalembela kuti : “ Musapeleke ziwalo zanu ku ucimo kuti zikhale zida zocitila zinthu zosalungama , koma dzipelekeni kwa Mulungu monga anthu amene auka kwa akufa . Ziwalo zanunso muzipeleke kwa Mulungu monga zida zocitila cilungamo . ” Amayang’ana anthu oipa ndi abwino omwe . ” — MIY . ( Ekisodo 23 : 25 ; Deuteronomo 7 : 15 ) Ena anawacilitsa . ( b ) Kodi Yehova anacita ciani kuti akwanilitse cifunilo cake ? Kumeneko , Kyoko anapeza anthu ambili amene anali kumumvetsetsa ndi kumuganizila . 9 : 11 , 12 ) Kodi Yehova amathandiza bwanji anthu kuyanjananso naye masiku ano ? Tingaonetse kuti ndise anzelu mwa kukhala na umoyo wosalila zambili , kupewa nkhongole zazikulu , kapena kugula zinthu zodula . Tikatelo , tidzatha kutumikila Mulungu momasuka , m’malo mokhala akapolo a anthu amalonda a m’dzikoli . — 1 Tim . Mungapeleke ndalama n’kufotokoza kuti mudzaziitanitsa mukadzazifuna . 5 : 19 - 21 ) Tifunikanso kudzifunsa kuti , ‘ Kodi nikupitiliza kuphunzila kuti nikhale watsopano mu mphamvu yoyendetsa maganizo anga ? ’ ( Aef . Yesu anacenjeza otsatila ake kuti : “ Anthu onse adzadana nanu cifukwa ca dzina langa , koma yekhayo amene adzapilile mpaka pa mapeto ndi amene adzapulumuke . ” — Mat . Mlembi wina anati : “ Kukamba zoona , kupatsa kumadalitsa nthawi zonse — malinga ngati tipeleka tilibe maganizo ofuna cotibwezela . ” Tsiku laciweluzo silidzatifikila “ ngati mbala ” ‘ tikakhalabe maso ndi oganiza bwino . ’ ( Onani cithunzi cili pamwamba . ) ( b ) N’ciani cimene tifunika kudziŵa ponena za fanizo la nkhosa ndi mbuzi ? Conco , iye sanali kukamba za nkhosa ndi mbuzi zenizeni . ( b ) N’ciani cimene mmela wa tiligu umabala ? 5 : 10 . Ndinaphunzila Kulemekeza Akazi ndi Kudziona Moyenelela 10 ( a ) Pamene Isiraeli anali wokhulupilika kwa Yehova , kodi mitundu yowazungulila inakhudzidwa motani ? Mfundo zimenezo zingakuthandizeninso kudziŵa mmene mungafotokozele zikhulupililo zanu kwa ena . Yelekezani kuti mukuona Sara akumwetulila uku akukamba kuti : “ Mulungu anandisekeletsa ine , onse akumva adzasekela pamodzi ndi ine . ” Tisanayankhe funsoli , tifunse kuti , mumacita ciani mukafuna kukambilana ndi bwenzi lanu limene limakhala kutali ? Kukamba zoona , uthenga woyela wocokela m’Baibulo ukadzala m’maganizo athu , ukhoza kutiyeletsa ndi kucotselatu zoipa zonse . Conco , tiyeni tikambilane ena mwa malangizo acikondi a m’kalata imene Paulo analembela Akhristu a ku Kolose . Ganizilani zimene Yehova anauza Yesaya kulemba za iye mwini . Iwo anandiitanila ku misonkhano ya mpingo ndipo ndinavomela . Sikuti Abulahamu anali wabodza kapena wamantha , monga mmene otsutsa amakambila . Nimayamikila maningi thandizo limene n’nalandila kwa abale okhulupilika Nidzaŵapatsa umboni woonetsa kuti zimene akamba n’zabodza . ’ Zofalitsa zathu zinali kufotokoza kwambili tanthauzo la ulosi wa m’Baibulo . 3 : 15 ) Patapita zaka zambili , mtumwi Paulo anayamikila Mulungu cifukwa ‘ cotimasula ndi dipo lolipilidwa ndi Kristu Yesu . ’ Umboni wa zimenezi ni mavuto amene anabwela cifukwa ca kusadziletsa kwa Adamu na Hava . Cotelo tonsefe tiyenela kuwatsatila , kaya tili ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha kumwamba kapena padziko lapansi . Nazi zinthu zinayi zokuthandizani kuti ana anu akulitse cikhulupililo cawo : ( 1 ) Kuwadziŵa bwino ana anu . Kutumikila Mulungu ndi “ mtima wathunthu ” kumatanthauza kudzipeleka kwa iye ndi mtima wonse kosalekeza . 10 , 11 . ( a ) Kodi Yesu anakonzekeletsa ophunzila ake kaamba ka nchito yotani ? Apa angaphunzilepo zinthu ziŵili zofunika . 15 : 20 , 23 . Mwacitsanzo , mlongo wina ku Norway mwamuna wake atafa mwadzidzidzi , anatsala yekha ndi mwana wake wa zaka ziŵili . Iwo ali ‘ pamalo otelela . . . mapeto ao ndi oopsa . ’ ( Sal . Timalandila thandizo la mzimu woyela wa Mulungu . Mwacionekele , apa n’kuti Baibo yonse italembedwa kale , ndipo patapita zaka zambili kucokela pamene Yesu anali padziko lapansi . N’zolimbikitsa kwambili kuona anthu ambili ocoka m’maiko ena akugwila nchito yokolola pamodzi ndi abale ndi alongo a ku malo osoŵa . Akristu odwala amam’tamanda mwa kulalikila pafoni , kulemba makalata , ndi kulalikila kwa owayang’anila ndi obwela kuwaona . Ciwawa ndi ciwelewele zili paliponse . Kodi Akristu ena amacita ciani kuti athandize okalamba mumpingo ? ( Aheberi 11 : 13 ) N’kutheka kuti pambuyo pake , adani a Inoki anafuna - funa mtembo wake , koma ‘ sanaupeze kwina kulikonse . ’ Mwina Yehova anabisa mtembo wa Inoki n’colinga cakuti anthu asauseŵenzetse pocilikiza kulambila konama , kapena kuugwilitsila nchito m’njila zina zolakwika . kwa anthu opita mu mseu . Ha , n’citsanzo cabwino cotani nanga cimene Yesu na Boazi anapeleka kwa akulu acikhiristu ! Koma M’bale Klein anayankha mosakondwa cifukwa anali wokhumudwabe ndi uphungu umene anapatsidwa . Kodi n’cifukwa cacitatu citi cimene cimatipangitsa kukhulupilila kuti Ufumu wa Mulungu ‘ udzabwela ’ posacedwapa ? Komabe ndinali kudana ndi malamulo amakhalidwe abwino a m’Baibulo . Conco ndinacoka n’kukakhala ndi mkazi wina amene ndinatomela . Ena sanali odzozedwa . M’zaka za m’ma 1900 , fodya unapha anthu 100 miliyoni . ( b ) Nanga makolo ali ngati abusa m’njila iti ? ( b ) Kodi makolo ozindikila angathandize bwanji ana awo ? Kodi “ Mapeto a Dziko ” ​ — N’ciani ? Mkristu aliyense payekha “ ayese nchito yake , kuti aone kuti ndi yotani . ” Kodi nkhani ino idzayankha mafunso ati ? N’ciani cimene tikuphunzilapo pa cozizwitsa cimeneci ? Patapita nthawi , anatumidwa kukatumikila ku Beteli ya ku Malawi . Kenako , Federico anacita chimo . ( Yow . Mwacitsanzo , anthu sanali kuloledwa kukhala ndi Baibulo kapena kuliŵelenga m’cinenelo cimene angamvetsetse mosavuta . Conco , mtsikana ameneyu anali kufunikila kwambili citonthozo na cilimbikitso . Atayamba kugwilitsila nchito Nsanja ya Mlonda yokhala ndi cingelezi cosavuta kumva , iye analemba kuti : “ Panopa ndimayankhapo maulendo angapo , ndipo mantha anathelatu . M’malo mofunapo ulemelelo wake , Mose anaonetsa kuti akanakonda mphatso zauzimu zimenezo zikanapatsidwanso kwa atumiki onse a Yehova . Howard anakamba kuti : “ Kuyambila capakati pa zaka 100 zoyambilila , Baibo ya Septuagint inakhala ya machechi achikhristu . Amishonale a machechiwo anali kuyenda m’masunagoge ‘ kufotokoza ndi kusonyeza umboni wolembedwa wakuti Yesu ndiye Mesiya . ’ ” Ponena za cosankha cake , iye anati : “ Sindimalakalaka umoyo wanga wakale ndipo ndili ndi cimwemwe cacikulu kwambili masiku ano . Iye anakamba kuti anthu amene ali ndi ciyembekezo cokakhala kumwamba ndi “ kagulu ka nkhosa , ” ndipo amene ali ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi ndi “ nkhosa zina . ” ( Aheberi 10 : 39 ) Ndipo tifunika kucita zimene tingathe kuti tilimbitse cikhulupililo cathu . Pali kusiyana pakati pa kukhala na cizoloŵezi ca khalidwe loipa limene lingafunike kulithetsa , na kulakwitsa kumene kungafunikile cabe kum’thandiza kuti azindikile zimenezo . ” — Wendell . 133 : 1 - 3 . Kodi anthu otalikilana na Mulungu amaonetsa cikondi cotani ? Mwamuna wake anauza abululu ŵake kuti mkazi wake wapempha kupita ku “ msonkhano wa Mboni , ” ndiyeno adzabwela ku cikondwelelo msonkhano ukatha . Iwo anakamba kuti , “ Basi sabwela , cifukwa Mboni za Yehova sizicita cikondwelelo ca tsiku la kubadwa . ” Koma pofika kumapeto kwa ma 1800 , maboma ambili sanali kucilikizanso machechi . Kodi Ophunzila Baibo analimba mtima na kutenga kaimidwe kotani cifukwa ca kupatulika kwa moyo ? “ Tsopano tadziŵa zimene anthu akufunikila kuti akhale ndi moyo . Sikuti ndi nchito kapena ndalama , koma cakudya . Nawonso alongo acikulile ni dalitso mumpingo . Musaiŵale kuti Yesu anati : “ Tangotsimikizani kuti mukati Inde akhaledi Inde , ndipo mukati Ayi akhaledi Ayi . ” Kuti mudziŵe zambili za mmene Baibulo lingakuthandizileni , onani kabuku kakuti A Satisfying Life ​ — How to Attain It , kofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . Kapezekanso pa www.jw.org Iye anati : “ Kuganizila kuti Yehova ndi ‘ Mulungu wacimwemwe , ’ kunandithandiza kuona kuti aliyense akhoza kukhala ndi cimwemwe kaya ali m’cikwati kapena ai . Kukambilana zimenezi kudzatithandiza kudziŵa mmene tingaonetsele kuti timakonda ndi kuyamikila Atate wathu wacikondi wakumwamba , amene amatiphunzitsa kuti tipindule . — Yes . ( Aheberi 6 : 19 ) Ndipo Mulungu “ wapeleka citsimikizo kwa anthu onse mwa kumuukitsa [ Yesu ] kwa akufa . ” — Machitidwe 17 : 31 . Maganizo ake amangosumika pa kuyendetsa bwino udindo umene ali nawo , ndi kusangalala nawo , cifukwa couona kuti ni wocokela kwa Yehova . Mtumiki wina wa Yehova amene ndi ciyamba kale anafotokoza malingalilo ake motele : “ Mboni zimayesetsa kusunga gulu la Yehova kukhala loyela ndi losadetsedwa . Ndipo cilango cimapelekedwa kwa aliyense amene walakwa . ” Ndinakhuzidwa kwambili cakuti sindinathenso kucita mapemphelo a namazi . Tingakhale bwanji mogwilizana ndi pempho lathu lakuti cifunilo ca Mulungu cicitike pa dziko lapansi ? Poyamba , msilikaliyo sanakhulupilile zimenezo , ndipo anaganizila Alexandra kuti anali m’gulu la okuba anthu . Kodi Mulungu amatipatsa cakudya ca kuuzimu m’njila yotani ? 118 : 6 , 7 ) Nkhani ino ifotokoza zinthu zinai zimene zionetsa kuti Mulungu amatikonda . Nanga n’cifukwa ciani na ise tifunika kukhala odekha pa zocitika zaconco ? Kodi izi ziyenela kutisoŵetsa cimwemwe ? Komabe , pakubuka mafunso angapo : Kodi pali maumboni ena ati oonetsa kuti m’zaka zambili zokafikitsa ku 1914 , odzozedwa anali kumasuka mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu ? Ucimo umatisonkhezela kucita zoipa . Komanso umatilepheletsa kucita zinthu zimene tidziŵa kuti ndiye zabwino , kapena zimene tiona kuti tingazikwanitse . Nanga bwanji ifeyo masiku ano ? 3 : 9 ) Ndife oyamikila cotani nanga , kukhala na mwayi wolambila Yehova mogwilizana ! Kuwonjezela apo , anagwilitsila nchito mwayi umenewu kulimbikitsa abale . ( Mac . Tinali kugwila nchito yoyeletsa m’khicheni , ndipo tinali kulema kwambili . Ganizilani za ana a Aroni , Nadabu ndi Abihu , amene anaphedwa cifukwa cofukiza “ pamoto wosaloledwa , ” mwina cifukwa cakuti anali okolewa . ( Lev . 4 : 18 . Pokhala mkazi wacikondi , iye ayenela kuti anali ndi azilongosi ake , ana aamuna ndi aakazi a azilongosi , azakhali , ndi azimalume ake , amene anali kuwakonda kwambili , komanso amene mwina sakanawaonanso . Mlongo wina wa zaka 79 dzina lake Inge , amene ali ndi vuto la maso , amakonzekela misonkhano pogwilitsila nchito mapepala a zilembo zazikulu amene m’bale wa mumpingo wao amamusindikizila . Tikakumana ndi anthu amene anasokeletsedwa ndi cipembedzo conama kapena amene amatsatila miyambo yacikunja , timawalankhula mwaubwenzi ndi mwamtendele . Akristu amene amasamukila kumalo osoŵa kapena kuphunzila cinenelo catsopano , nthawi zambili amakhala ofalitsa aluso ndipo amathandiza kwambili kuti mpingo upite patsogolo . Kodi wacicepele angathe kukhala wokhwima mwakuuzimu ? Mwacionekele , Yehova anaona zimenezi , ndipo anatithandiza cakuti tsikulo ndi losaiŵalika kwa ife . Tili ndi zifukwa zambili zokondela Yehova ndi mtima wonse . M’kupita kwa nthawi , zinenelo zimasintha , moti mau amene poyamba anali kutanthauza zinthu zina angasinthe kwambili n’kuyamba kutanthauza zinthu zinanso . ( Mat . 24 : 14 ) Ndiyeno , asanakambe za nkhosa ndi mbuzi , Yesu anapeleka fanizo la matalente pofuna kuphunzitsa odzozedwa kuti afunika kugwila nchito yolalikila mwakhama . Tumikilani Mulungu Mokhulupilika Panthawi ya “ Masautso Ambili ” Kuti Yehova atithandize , tiyenela kukhala pamalo pamene mzimu wake umapezeka , monga pamisonkhano ya mpingo . Baibulo limakamba kuti “ anthu osadziŵa zinthu , ndithu adzakhala opusa , koma kwa ocenjela , kudziŵa zinthu kudzakhala ngati covala ca kumutu . ” — Miyambo 14 : 18 . Tizithetsa Mikangano Mwamtendele , May Cifukwa ca zimenezi , ndinayamba kudana kwambili ndi Mboni za Yehova . ” Tisaiŵale kuti tanthauzo la maulosi a m’buku la Danieli anali cinsinsi mpaka “ nthawi ya mapeto . ” Pothela pake , tsiku limene tafotokoza kuciyambi kwa nkhani ino linafika . Atumiki ake amakhala acimwemwe cifukwa amakonda kuthandiza ena . Kumeneko anali kugwila nchito pa famu ndipo anali kum’zunza monga kapolo . M’malo motsanzila citsanzo cake cabwino io anamuuza mau ofooketsa kuti : “ Udzabwelanso kuno posacedwa . Ngati tipitiliza kucita zimenezi , Yesu adzatiweluza monga nkhosa ndipo tidzaona kukwanilitsika kwa mau ake akuti : “ Bwelani , inu amene mwadalitsidwa ndi Atate wanga . Loŵani mu ufumu umene anakonzela inu kucokela pa kukhazikitsidwa kwa dziko . ” — Mateyu 25 : 34 . Koma ife tikamacilikiza ulamulilo wa Yehova , timaonetsa kuti tili kumbali ya Mulungu . Naine nimafuna kukhala na ziwalo zonse . Tidziŵa cifukwa cakuti Yesu anakaniwa kuti si Mesiya ndipo anaphedwa . Yesu anali kulikonda dzina la Yehova . ( Yoh . N’zolimbikitsa kwambili kuona mmene Yehova akutisamalila pamene tikutumikila m’gawo losoŵa . ” ( Sal . NTHAWI zonse kukonzekela mwambo wa cikwati kumatenga nthawi yaitali . Zoonadi , “ makhalidwe [ a Mulungu ] osaoneka ndi maso akuonekela bwino . Makhalidwe a Mulungu amenewa , ngakhalenso mphamvu zake zosatha ndiponso umulungu wake , zikuonekela m’zinthu zimene anapanga . ” — Aroma 1 : 20 . Anthu ena amacita zinthu zimene Mulungu amazonda , koma n’kumadzinenela kuti amalambila Mulungu . M’bale wina wa ku Brazil anakamba kuti , “ Pa zaka 23 zimene takhala m’cikwati , takhala na umoyo wosangalala kwambili cifukwa ine na mkazi wanga timakonda zinthu zauzimu . ” 37 : 18 , 19 ) Kodi lonjezo limeneli lakwanilitsikadi masiku ano ? Mungacite bwino kuganizila zina mwa zinthu zimene iye watipatsa cifukwa cotikonda . N’cifukwa ciani Paulo , munthu “ wokhwima ” kuuzimu amene mwina anali m’bungwe lolamulila m’nthawi ya atumwi , anadzicha kuti “ munthu wovutika ” ? Cuma Camasiye : Mukhoza kulemba mu wilo yovomelezeka ndi boma kuti gulu la Yehova lidzapatsidwe katundu wanu kapena ndalama zanu , inuyo mukadzamwalila . Ndimaganizila lemba la Mateyu 5 : 23 , 24 ndi kuona zimene ndingacite kuti ndithetse mikangano . Arthur analibe nthawi yokwanila yokonzekela nkhani zake . Koma mtima wake wodzipeleka kucita nchito zovuta potumikila Yehova , unali kunilimbikitsa ngako . Mau akuti “ Yehova mmodzi ” amatithandiza kumvetsetsa kuti Yehova afuna kuti atumiki ake azigwilizana ndi kukhala ndi colinga cimodzi . Iweyo ukhala woyang’anila nyumba yanga , ndipo anthu anga onse azimvela iweyo . Mwacionekele , n’cifukwa cakuti anali munthu wauzimu . Ine ndi mkazi wanga , timakondwela kuthandiza ena kuphunzila Baibulo . Pankhani yosankha zosangalatsa , kodi tiyenela kukumbukila mfundo ziti ? N’cifukwa ciani anali otsimikiza za zimenezi ? Komabe , timadziŵa kuti mwai wodziŵika ndi dzina la Mulungu limeneli umafuna kucita zoonjezeleka . Kuphunzila Baibulo ndi kwaulele ndipo mungaphunzilile panyumba panu kapena pamalo aliwonse amene mufuna . Yesu ananenanso za gulu laciŵili la anthu okhulupilika amene adzapindula ndi madalitso a Ufumu wa kumwamba . Pa msonkhanowo , Petulo anakamba molimba mtima . Iye anakumbutsa abale kuti m’zaka zam’mbuyo , anthu amitundu ina osadulidwa , analandilapo mphatso ya mzimu woyela . Lemba la caka ca 2018 : “ Anthu odalila Yehova adzapezanso mphamvu . ” — YES . 12 , 13 . ( a ) Kodi mbuye adzauza ciani akapolo aŵili oyamba ? Nanga cifukwa ciani ? Iyai . Kukhala wokhulupilika kwa Mulungu cinali cinthu cofunika kwambili pa umoyo wa Yonatani . Mungadziŵe zimene munthu amakhulupilila kokha mutafunsa munthuyo mwacindunji . Pafupifupi zaka 2000 zapitazo , Yesu Kristu ananena za ngozi imene inapha anthu 18 pamene nsanja inawagwela . Kodi ndimafunafuna mipata imene ndingaonjezele utumiki wanga kwa Yehova ? ’ Anthuwo anauza Milan na mng’ono wake kuti akwele m’motoka yawo kuti adutse nawo paboda , cifukwa ziphaso za ana sanali kuzifuna . Koma cimene cinawalimbikitsa kwambili n’cakuti abale oimilako gulu la Mulungu anabwela kudzayendela mpingo wawo . Nditadziŵa kuti Wamphamvuyonse ndi amene ali ndi mphamvu pa moyo ndi pa imfa , ndinayamba kumucondelela tsiku lililonse kaamba ka umoyo wa atate anga . ( Gen . 11 : 31 ; Aheb . 11 : 8 , 9 ) Abulahamu sanali kukhulupilila kuti angatetezedwe ndi mafumu aumunthu kapena mizinda yamipanda . Angelo ena miyanda miyanda amatumikila Mulungu monga nthumwi pocita cifunilo cake . Atate anafika pokhala mnzanga wapamtima , ndinali womasuka kukamba nao . Pamene Yesu anali wacicepele , mwacionekele anavutikapo na cisoni cifukwa ca imfa ya acibululu kapena mabwenzi ake . Pambuyo pake , ananiuza kuti adzanilemba . Cifukwa cophunzila Baibulo , iye anazindikila kuti afunika kusintha mmene amamvelela cifukwa ca zimene abale amalakwitsa . Mulungu “ anapeleka Mwana wake wobadwa yekha . ” Zimene zinacitikila mlimi wina amene anali kucita lendi malo olimapo m’dela la mapili ku Masbate m’dziko la Philippines , zionetsa kuti Yehova amatsogolela . Koma pali mfundo zina zimene zingatithandize kuwongolela kaimbidwe kathu . Komabe , ufulu wathu ungakhale “ cophimbila zoipa ” ngati timakhala akapolo a zilakolako za thupi lathu , kapena ngati timangotengela masitaelo onyazitsa a dziko lino . Mwacitsanzo , Mkhristu mnzathu akasoŵa zinthu zofunikila pa umoyo , tingafunike kum’thandiza , osati kungokamba mau a mafuno abwino . Conco , iye amacoka pagalasi popanda kukonza zolakwika . Tidzakhala ndi mwai wophunzitsa anthu oukitsidwawo cifunilo ca Mulungu ndi colinga cake . Mwa kucita zimenezi tidzawathandiza kuti ayenelele kukhala ndi “ moyo wosatha . ” — Mac . 24 : 15 ; Yoh . 17 : 3 . Akhiristu amene analemba Baibo anaonetsa kufunika kwa cikhulupililo mwa kucitomola kambili . Kumeneko , n’nakumananso na wacicepele wina , dzina lake Juan Ardanez , amene mofanana ndi anthu a ku Bereya , anali kufufuza mosamala kuti aone ngati zimene anali kuphunzila m’Baibo zinali zoona . ( Mac . Angafunsilenso za mapindu ake na ciopsezo cimene cingakhalepo kwa mkazi . Kucita zimenezo kunawathandiza , ndipo anasamukila ku Ghana mu 2004 . Yembekezelanibe ! ( b ) Nanga amatiphunzitsa ciani za colinga cake kwa ife ? Ngati zimenezi n’zoona , kodi m’dziko mukanakhala mavuto ambili conco ? TSAMBA 7 • NYIMBO : 108 , 129 Tiyenela kudziŵa zambili mwa kufufuza . Cinandisangalatsa kwambili n’cakuti anali kuŵelenga nkhani ina yomwe si yophunzila , koma anali kuŵelenganso malemba . Ngakhale kuti Yesu anali kudziŵa kuti adzaukitsa Lazaro , anakhudzidwa kwambili ataona cisoni cimene Mariya na Marita anali naco . Tingaonetse kuti tikufunitsitsa kudzakhala ndi moyo weniweni mwa kukonzekela tsopano . Monga mmene citsanzo ca Jordan cionetsela , anthu ena angaone kuti mphatso ina yake ni yosathandiza konse . Aliyense mumpingo ali ndi udindo wogwila nao nchito zimenezi . Iwo anazunzidwa mwankhanza cifukwa colalikila uthenga wa Ufumu . ( Mac . 1 : 5 ) Komabe , nchito yolalikila padziko lonse inafunika citsogozo ndi dongosolo . Zimenezi “ zinawatonthoza kwambili . ” — Mac . 20 : 7 - 12 . Ena m’banja angakhumudwe ngati wacibale wasankha kusapita ndi kusiya banja lake kapena wasankha kubwelela kunyumba . N’zoona kuti polaila anachulako zopita kucipatala , koma kodi tinganene kuti munthuyo anali woona mtima , kapena cinali cinyengo ? 3 : 36 ) Cikhulupililo ca Mkhiristu cimaphatikizapo kuonetsa kuti timamvela malamulo a Yesu . Cilengedwe cimationetsa kuti palibe angapose Mulungu pa nkhani ya dongosolo . Kodi Ulamulilo wa Yesu wa Zaka 100 Wakupindulitsani Bwanji ? * Conco , muyenela kupempha Yehova kuti akuthandizeni . Munthu amene timakonda akamwalila , timamva cisoni , koma timakhala ndi ciyembekezo . Koma posakhalitsa , n’naima upainiyawo kwa kanthawi . Kuti mapemphelo athu aziyankhidwa , tiyenela kupemphela kwa Mulungu wochulidwa m’Baibulo , Yehova , * osati kwa mulungu wina kapena kwa makolo amene anamwalila kalekale . NCHITO yofunika kwambili imene ikugwilidwa padziko lapansi masiku ano ndi yolalikila uthenga wabwino . Nafenso , nthawi zina zingativute kupanga cosankha cifukwa cosadziŵa bwino - bwino njila yoyenelela . ( Mat . 12 : 50 ) Cinanso , iwo ali m’banja lalikulu lauzimu , la anthu ogwilizana cifukwa ca cikondi na cikhulupililo . M’nthawi ya atumwi , Yohane anaona masomphenya a angelo 7 amene anali kuliza malipenga . Kodi ndi kusintha kotani kumene kwacitika m’gulu la Mulungu kocokela pamene Ufumu unakhazikitsidwa ? Mwa kupeleka moni , tingathandize ena kudziona kuti ni ofunika pakati pa anthu a Yehova . Nanganso zokamba zathu , kodi zimalemelela ku ciani ? “ CIMENE ndinabadwila ndiponso cimene ndinabwelela m’dziko ndico kudzacitila umboni coonadi . ” ( Ŵelengani Salimo 97 : 10 . ) Zimakhala zovuta kwa io kupewelatu fungo la pelefyumu cifukwa amakumana ndi anthu osiyanasiyana tsiku ndi tsiku . ( Ŵelengani Luka 21 : 36 . ) Mulungu amadziŵa kufooka kwathu ; “ amakumbukila kuti ndife fumbi . ” ( Sal . 6 , 7 . ( a ) Fotokozani colinga ca ubatizo wa Yohane . ( b ) Ni ubatizo wapadela uti umene Yohane anacita ? 3 : 18 ) Kucita zimenezi kumafuna khama . Liuli silinena za mphepo wamba . . . koma limanena za cimphepo coopsa camkuntho , cophatikizapo cimvula camphamvu ndi mitambo yakuda bii , cimene cingaononge zinthu kwambili . ” — Mat . 5 : 23 . Zingakuthandize kuti cikhulupililo cako cikhale monga mtengo wa mizu yofika patali . Nanga n’cifukwa ciani anakukila ku Myanmar ? Kuwonjezela apo , nthawi zina olamulila amacititsa kuti abale na alongo avutike kugwilizana na mpingo . ( 2 Petulo 3 : 9 ) Kodi mudzayamikila cikondi ca Mulungu ndi kumvela cenjezo lake ? Ufumu wa Mulungu ndi boma lenileni limene likulamulila kucokela kumwamba . Iye anali kudziŵa kuti colakwa cimodzi cikhoza kutsogolela ku cina , mpaka munthu angafike pocita chimo lalikulu . Zimene Samuel , Teresa , ndi Magdalene anakamba zikuonetsa kuti anthu amapemphela pa zifukwa zosiyanasiyana , ndipo zifukwa zina ndi zomveka koma zina sizomveka . COLINGA CA MLENGI Buku la m’Baibulo la Genesis , limatiuza mwatsatanetsatane mmene Mulungu analengela dziko lapansi . Pamenepa , m’baleyu anazindikila kuti anacita bwino kwambili kukhala wodekha panthawi imene munthuyo anali kumunyoza . Posapita nthawi , tinadziŵana na abale na apainiya , komanso tinalidziŵa bwino gawo . ” Mu May 2007 , Daniel na Miriam , analeka kuseŵenza , n’kupita ku dziko la Panama , kumene m’mbuyomu , anapita kukayenda . ( Tito 2 : 10 ) Ndipo tikakhala oona mtima , Mulungu sangatisiye . Iye anali wokhulupilika kwa mwamuna wake , cikwati cake , ndi kwa Mulungu wake . N’ciani cinathandiza Danieli na wolemba Salimo 119 kukhalabe auzimu ? 25 : 8 - 12 ) Conco , lamulo la Aroma linathandiza “ pa kuteteza uthenga wabwino ndi kukhazikitsa mwalamulo nchito ya uthenga wabwino . ” — Afil . Malinga ndi Salimo 15 : 3 , 5 , kodi Mulungu amafuna kuti tizicita ciani kuti tikhale naye paubwenzi ? Ngakhale n’conco , nchito imene io amapatsidwa nthawi zonse imalemekeza Yehova , ndi kupindulitsa anthu okhulupilika . Buku lina limati : “ Kale ku Isiraeli kunali nkhalango zikuluzikulu kusiyana ndi masiku ano . ” Tidzaphunzilanji m’nkhani ino ? Nanga akumanapo ndi zotani ? YELEKEZANI kuti mufuna kundandalika malemba amene Mboni za Yehova zimakonda kuwaseŵenzetsa . Pambuyo pa caka cimodzi , n’nayamba kutumikila monga wothandizila m’Komiti ya Utumiki ya Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova . Kodi pali ciliconse cimene tingacitepo ? M’nthawi zakale , mzinda wa Babulo unali likulu la zamalonda . THANZI LABWINO NA KUPILILA Mu 1980 , ndinakaloŵa m’kalabu ya oponya zibakela ku Beirut . Muzigona mokwanila . Ndipo anthu ambili kumeneko , kuphatikizapo acibale anga , sanali kukhulupilila kuti Mulungu aliko . Caka cotsatila , m’dzikolo munacitika misonkhano iŵili yacigawo , wina mumzinda wa pafupi na doko wochedwa Veracruz , wina ku Mexico City . Nanga zinthu zinamuyendela bwanji atasamuka ? 2 MUZISINKHA - SINKHA . M’malo mwake , anapempha kuti apatsidwe nchito imene siinali kukhudzana ndi usilikali . 20 : 12 ; Aef . Satana sanalengeko cinthu ciliconse . Paulo anayamikila mfundo imeneyi , ndipo anakamba kuti : “ Mulungu waonetsa kukoma mtima kwake kwakukulu kumene kumabweletsa cipulumutso kwa anthu , kaya akhale a mtundu wotani . ” — Tito 2 : 11 . Zipembedzo zina ndinazionanso kuti n’zopanda phindu . N’ciani cionetsa kuti Mariya anali munthu wauzimu ? Conco ndinaganiza zopitiliza kutumikila . Ndipo naonso akulu anali kudziŵitsa abale amene ayamikilidwa kumene , ndi kuwafunsa ngati ndi okonzeka ndi oyenelela kulandila udindo umenewo . 7 : 9 ) Mbili imeneyi ionetsanso kuti Mulungu nthawi zonse amasunga malonjezo ake . Koma ine ndi banja langa tinalimbana ndi vuto la zacuma limeneli mwa thandizo la Mulungu . ” Musabwezele coipa , . . . pakuti Malemba amati : ‘ “ Kubwezela ndi kwanga , ndidzawabwezela ndine , ” watelo Yehova . ’ ” Iye anakamba kuti anali kuopa kukatumikila ku malo osoŵa cifukwa coganiza kuti sangakwanitse . Koma ena a ife amene tikaliko ndi mphamvu , tizikumbukila mau ouzilidwa akuti : “ Kumbukila Mlengi wako Wamkulu masiku a unyamata wako , asanafike masiku oipa . ” — Mlal . Muziganizila Malemba amene adzakuthandizani kupewa kutenga mbali m’zandale . Cinanso , mfundo yakuti anthu angakwanitse kuthetsa mavuto awo ingaoneke ya zoona kwa ena , cifukwa kafuku - fuku waonetsa kuti nkhondo , upandu , matenda , ndi umphawi , lomba zikucepekela . Kupempha Mphamvu “ Ndiceukileni ndi kundikomela mtima . ( Rute 1 : 16 , 17 ) Iye anali woona mtima , ndipo anagwila nchito yokunkha mwakhama potsatila makonzedwe a m’Cilamulo ca Mose othandiza anthu osauka . Ndi kutinso : “ Molingana ndi mphatso imene aliyense walandila , igwilitseni nchito potumikilana monga oyang’anila abwino . ” ( Agal . 6 : 10 ; 1 Pet . Makalatawo anali opempha abale ndi alongo aluso kuti afunsile utumiki wa kanthawi pa Beteli , ndi kukathandiza panchito yomanga nyumba zina za Beteli ku Wallkill , New York . Ezekieli anamvela phokoso lakuti “ gobedegobede . ” Yosimbiwa na Denton Hopkinson Komabe , tisazengeleze kukaniza ziphunzitso zilizonse zosagwilizana ndi malemba . Atate anali munthu waubwenzi kwambili , koma ndinali kudabwa cimene cinali kuwacititsa kukwiila alongo ao amene anali okoma mtima . Mofanana ndi Cesar ndi Rocio , abale ndi alongo ambili asintha zinthu zina kuti athandize panchito yomanga imene ikucitika ku New York . Olemba Baibulo analemba mau ocokela kwa Yehova ndi mbili yokhudza ubwenzi wa pakati pa Mulungu ndi anthu ake . Mlongo wina amene ni mpainiya anacelezapo abale na alongo oloŵa masukulu ophunzitsa Baibo . Iye anati : “ Poyamba n’nali kuyopa kulandila alendo cifukwa nyumba yanga ni yosaukila ndipo muli mipando yakale imene ena ananipatsa . ( Aroma 1 : 20 ) Iye analenga dzikoli m’njila yakuti tizisangalala ndi moyo . Kuti tikondweletse Yehova , tonse tinaona kuti tifunika kusintha khalidwe lathu loipa kuti tilele bwino mwana wathu . Komabe , iye ndi mkazi wake anavutika ndi cikumbumtima . Kodi tingaonetse bwanji ulemu kwa mwininyumba ? Cifukwa cakuti bodza ni cimodzi mwa zida zamphamvu zimene Satana amaseŵenzetsa . 1 : 3 , 4 . 17 - 19 . ( a ) Tingadziŵe bwanji kuti cikhulupililo cathu n’colimba ? Posacedwa , Monique anakhala na mwayi woloŵa Sukulu ya Alengezi a Ufumu . Ndi vuto lotani limene linabuka mumpingo wa ku Korinto ? Sikudzakhalanso ngozi zacilengedwe . 5 : 18 - 21 . Kuwonjezela apo , n’nali kukhulupilila kuti cuma conse cifunika kugaŵidwa mosakondela , kuti pasakhale olemela kwambili kapena osauka . Mphatso zimenezi zocokela kwa Yehova zimatilimbikitsa kupitiliza kubala zipatso . — Yak . Cikondi cimeneci cikutanthauza kuti ife sitinakonde Mulungu , koma iye ndi amene anatikonda ndi kutumiza Mwana wake monga nsembe yophimba macimo athu . ” — 1 Yoh . 4 : 9 , 10 . ( Akol . 3 : 12 ) Thomas anazindikila kuti mwana angafunike kukamba naye nkhani zina mobweleza - bweleza kuti afike pokhutila . Mwacitsanzo , Helena wa zaka 71 , wa ku Mozambique anakamba kuti : “ Ndine waubwenzi ndipo ndimalemekeza anthu ena . “ Aliyense . . . akonde mkazi wake ngati mmene amadzikondela yekha , komanso mkazi azilemekeza kwambili mwamuna wake . ” — AEF . M’malo moona kuti nkhani zimenezi zimangogwila nchito ku gulu limodzi la anthu , anthu Mulungu kuyambila kale , kaya ndi odzozedwa kapena ai akhala akugwilitsila nchito mfundo zambili zimene amaphunzila m’nkhani za m’Baibulo . Ifenso tikucitila umboni , ndipo iwenso ukudziŵa kuti umboni umene timapeleka ndi woona . ” ( 3 Yoh . Anali kuwacezela kaŵilikaŵili m’madzulo ndi kumamvetsela mavuto ao ndiponso kuwalimbikitsa . Koma ngati mwaona kuti pali cifukwa comveka cokambila naye , muyenela kuyembekezela mpaka mtima wanu utakhala pansi . 60 : 5 ) Timaona umboni wa zimenezi tikaona kuculuka kwa anthu amene amapezeka pa misonkhano yathu ya cigawo ndi pa Cikumbutso caka ciliconse . Ndithudi , iwo ni zitsanzo zabwino pa nkhani yoseŵenzetsa ufulu wathu potamanda na kulemekeza Mulungu wathu waufulu , Yehova . Masiku ano , Yehova wapitilizabe kucita zinthu mogwilizana ndi dzina lake , mwa kusamalila zosoŵa zathu zakuthupi , ndi zakuuzimu . Kodi lomba tidzakambilana mafunso ati okhudza kuuka kwa akufa ? Mulungu Amayankha Mapemphelo Onse ? Yehova angakuthandizeni kuona makhalidwe abwino mwa ana anu acinyamata . N’cifukwa ciani cakudya cakuuzimu n’cofunika kwambili ? Iwo anali kudziŵa kuti kucita mwambowo kunali kosagwilizana ndi zikhulupililo zanga ndi za mkazi wanga . Conco pambuyo pokambilana kwa nthawi yaitali io anakacitila kwina mwambo umenewo . Zingakhale bwino nditangosiya kugwila nchitoyi . ’ ( Ŵelengani 2 Samueli 7 : 12 , 16 . ) Pamsonkhano umenewo anafunsa banja lina la amishonale limene linali kutumikila ku Taiwan . Ndiyeno , pamene ana anali kubadwa , ‘ imfa inafalikila kwa anthu onse . ’ Aliyense payekha afunika kuphunzitsa cikumbumtima cake kuti cizimutsogolela mogwilizana na miyezo ya Mulungu . N’cifukwa ciani tiyenela kuyembekezelabe mapeto a dziko loipali ? Tili ndi masukulu ena ambili monga , Sukulu ya Utumiki wa Ufumu , Sukulu ya Apainiya , Sukulu ya Alengezi a Ufumu , Sukulu ya Oyang’anila Oyendela ndi Akazi ao , ndi Sukulu ya a m’Komiti ya Nthambi ndi Akazi ao . Ndi cofalitsa cofunika citi cimene tifunika kusinkhasinkha ? Ndipo kucita zimenezi kudzatithandiza bwanji ? Ndipo , Mulungu amafunitsitsa kudziŵa zimene tiganiza , cifukwa amafuna kuti tikhale paubwenzi wolimba ndi iye . 1 / 1 Lambilani Yehova , Mfumu Yamuyaya , 1 / 1 Tifunika kukumbukila kuti : “ Onse ndi ocimwa ndipo ndi opelewela pa ulemelelo wa Mulungu . ” Ofalitsa magazini imeneyi komanso anthu ambili amene amaiŵelenga , sakaikila zakuti nthawi yapadela imeneyi ndi masiku otsiliza ndipo mapeto ali pafupi kwambili . N’ciani cimaonetsa kuti Mulungu amatisamaliladi ? 30 Kodi Kukwatiwa “ Mwa Ambuye ” — N’kofunikabe ? N’kutheka kuti Nowa sanamvetsetse zambili zokhudza ulosi wa pa Genesis 3 : 15 . Ngakhale kuti zinthu zimenezi sizinapangidwe ndi anthu a Yehova , io amazigwilitsila nchito kupanga Mabaibulo ndi zofalitsa zina m’zinenelo zambili ndi kulalikila padziko lonse lapansi . Kodi mungadziteteze bwanji ? Koma cimene tidziŵa n’cakuti , Inoki , “ anayendabe ndi Mulungu woona . ” — Genesis 5 : 24 . 2 : 2 , 3 . ) Kodi Yesu asiyana bwanji ndi Adamu ? Mwacitsanzo , pokamba na anthu , muzimwetulila olo kuti poyamba simungafune kucita zimenezi . Ni abale na alongo athu mu mpingo . Ndithudi , iye amaona utumiki wake kukhala cuma camtengo wapatali . 10 : 25 ) Monga mmene Paulo anakambila kwa Akhristu a m’nthawi yake , na ise tikuti : “ Pitilizani kutonthozana ndi kulimbikitsana monga mmene mukucitila . ” — 1 Ates . N’nayamba kupemphela kwa Yehova Mulungu ndipo n’naleka kupepa fwaka . Zioneka kuti anthu ambili sasangalala ndi nchito yao cifukwa cakuti sacita khama kuti aidziŵe bwino nchitoyo . Masiku ano amacitanso cimodzimodzi , ndipo wacita kunyanyilatu . NKHONDO ZIDZATHA : “ Yehova . . . akuletsa nkhondo mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . VUTO : Amai Susan Rose - Ackerman , amene tawachula m’nkhani yapita anakamba kuti nchito yothetsa ziphuphu “ ifunika kuyambila kwa akuluakulu a boma . ” Davide anapempha Yehova kuti athandize Husai , ndipo Iye anam’thandizadi . Nthawi zambili timaganizila zimene Yehova adzaticitila m’Paradaiso . Koma m’nkhani ino , tidzakambilana zimene Mulungu adzacotsa padziko lapansi . Cikondi n’cofunika kwambili m’banja komanso pakati pa mabwenzi . Sindinali kudziŵa kuti io limodzi ndi ana ao aŵili anakhala a Mboni za Yehova . Tifunika kucita zinthu mmene Yehova amafunila . Kukhala mtsogoleli wa Aisiraeli cinali cinthu cofunika kwambili kuposa kukhala kalonga mu Iguputo . Ndithu musatelo ayi , koma pitilizani kulandila kukoma mtima kwakukulu ndi kumudziŵa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khiristu . ” — 2 Pet . Zonsezi zinayambitsa nkhani yofunika kwambili yakuti , kodi Mulungu ndi woyenelela kulamulila anthu ? ( 1 Maf . 11 : 5 - 8 ; 2 Maf . 23 : 13 ) Mwina Solomo anaganiza kuti Yehova adzanyalanyaza zolakwa zake malinga ngati apitiliza kupeleka nsembe pa kacisi . Ngakhale kuti Akristu ambili a zaka za m’ma 50 ali ndi mipata yocita zinthu zina zatsopano muutumiki wa Yehova , ena samakwanitsa kutelo . Iye “ anali wopanda colakwa pakati pa anthu a m’nthawi yake . ” Ambili a ife timafuna titakhala ndi nthawi yoculuka yoŵelenga Baibulo ndi zofalitsa zathu . Niona kuti cinthu cikulu cimene cacititsa kuti nipite patsogolo mwauzimu ni mmene n’naleledwela . ” Kuposa zonse , timatsatila citsanzo ca Yehova amene amaona anthu onse kuti ndi amtengo wapatali . A Yakobo , atate ake , sanadziŵe ciliconse cimene cacitikila mwana wao wapamtima , ndipo adzakhala akumuyembekezela madzulo . M’dziko lino lolamulidwa ndi Satana , amuna ndi akazi akumana ndi mavuto adzaoneni . ( Mlal . 8 : 9 ; 1 Yoh . Atumiki ena okhulupilika a Mulungu , ayamba khalidwe loipa cifukwa coceza ndi anzao a ku nchito amene si Mboni za Yehova akaweluka . “ Khulupilila Yehova ndipo cita zabwino . . . khala wokhulupilika m’zocita zako zonse . ” — Sal . Conco , nimayenda motsimphina moti nimalema mwamsanga . ” 1 : 8 ) Masiku anonso , Yesu salankhula mwacindunji ndi aliyense wa alaliki acangu a Ufumu oposa 8 miliyoni . Mkambi anawapempha kuti akhale pansi kuti amvetsele nkhani . Cifukwa caciŵili n’cakuti mukayamba kukwanilitsa zolinga zanu zauzimu , ndiye kuti mwayamba kudzipangila dzina labwino kwa Yehova . Tidzakambilananso mmene tingaonetsele makhalidwe amenewa pa nchito yathu yolalikila . Mau amunsi mu Baibo yakuti New World Translation of the Holy Scriptures — With References , analembedwa motsatila njila imeneyi . — wp17.4 , peji 11 - 12 . Mwacitsanzo , makolo athu oyamba anali kudziŵa kuti anafunika kucita zinthu monga kudya , kupuma , na kugona kuti akhalebe na moyo . Ine na Livija tingakambe motsimikiza kuti pa zaka zonse zimene takhala mu utumiki wa nthawi zonse , ‘ cimwemwe cimene Yehova amapeleka cakhala malo athu acitetezo . ’ — Neh . Mwacitsanzo , Faizal anaphunzitsidwa ndi makolo ake , amene sanali Akhiristu , kuti Baibulo ni buku yopatulika koma inasinthidwa . Zotsatilapo zake n’zakuti abalewo anakhazikitsa mtendele ndipo anaseŵenzela pamodzi pamsonkhano . Muziganizila za ciyembekezo cimeneci , muziciona kuti n’ceni - ceni , ndiponso muziuzako ena mwakhama za ciyembekezoci . Mwacitsanzo , kale kwambili Mose asanalembe lamulo la Yehova loletsa cigololo , Yosefe wacinyamata anadziŵa kuti khalidwe limeneli linali chimo kwa Mulungu . 2 : 20 ) Zoonadi , Timoteyo anali kuwakonda anthu . Kodi Mapeto a Dzikoli Ali Pafupi ? Pa 23 April caka cimeneco , M’bale Milton Henschel anakamba nkhani yopatulila maofesi atsopano amenewo ku gulu la anthu acimwemwe okwana 45,522 . Koma nthawi zina kucita zimenezi kumakhala kovuta . Monga mmene tinaonela m’nkhani yapita , Akristu oyambilila anapindula ndi lamulo laciroma limene linali kugwila nchito mu ufumu wonsewo . 12 : 1 - 17 ) Conco , tinali kukhulupilila kuti Gogi ndi dzina lina laulosi la Satana . Kodi Cilamulo ca Mulungu Cinali Kuvomeleza Kubwezela ? Zaka zambili zapitazo , mlongo wina dzina lake Stephanie , wa ku United States , amene lomba ali ndi zaka pafupifupi 30 , atapenda mmene zinthu zinalili pa umoyo wake , anati mumtima mwake : ‘ Nili ndi thanzi labwino ndipo nilibe udindo uliwonse wosamalila banja . Aphunzitseni kuyamikila zonse zimene Mulungu awacitila . ( Chiv . Zimenezo ndi umboni wakuti Mulungu amakondwela nanu , ndi kuti mzimu wake ndi ‘ wokhazikika pa inu . ’ Iye ananenanso kuti : “ Yehova Mulungu wanu ndiye Mulungu wa kumwamba ndi padziko lapansi . ” Kodi inu mumapemphela nthawi zonse ? Makolo anga atazindikila kuti sindidzatalika kuposa pamenepo , anandilimbikitsa kuti ndizigwila nchito kwambili kuti ndisamaganizile za msinkhu wanga nthawi zonse . Si copepuka kukhala ndi banja lolimba ndi lacimwemwe makamaka ‘ nthawi ino yovuta . ’ ( 2 Tim . Ngati ndife odzicepetsa ndi acangu mu ulaliki , ndipo ngati timacita phunzilo laumwini , tidzakhala ndi maganizo monga a Kristu . Pamene tikambilana , onani zimene acicepele ena anakamba za mavuto amene amakumana nawo povala cida ciliconse ca nkhondo yauzimu na mapindu amene amapeza . 9 : 26 - 28 ) Mpingo wa ku Yerusalemu utamva zimene Baranaba anafotokoza , unam’landila Paulo . NYIMBO : 81 , 135 N’zolimbitsa cikhulupililo kudziŵa kuti ngakhale ndise opanda ungwilo , tingathe kutumikila Yehova movomelezeka . Tikatelo , Yehova adzatidalitsa , tidzakhala osangalala tsopano , ndipo tidzapeza moyo wosatha m’dziko lake latsopano . — Yakobo 1 : 25 ; Chivumbulutso 1 : 3 . Kuonetsa cikondi cacikhristu kwa alendo ocokela m’dziko lina , kumakhala na zotulukapo zabwino . 7 : 9 , 14 ) Anthu amene adzapulumuka si “ khamu ” cabe koma ndi “ khamu lalikulu , ” anthu oculuka kwambili . M’nkhaniyo , muli malangizo akuti : “ Musafulumile kuganiza kuti mwana wanu sakugwilizana ndi zimene mumakhulupilila . Misozi inayamba kulenga m’maso mwa Katherine pamene a Doris anali kusimba cocitikaco . Kodi Akhiristu pa nthawi ina anakhalapo mu ukapolo molingana na Ayuda ku Babulo ? Mau a Mulungu amatithandiza kukhala ndi cidalilo cakuti ‘ onse amene ali ndi maganizo abwino amene angawathandize kupeza moyo wosatha ’ adzalandila uthenga wabwino . ( Mac . Poonetsa kufunika komvela mau a Mulungu , Yesu pa nthawi ina anati : “ Munthu sangakhale ndi moyo ndi cakudya cokha , koma ndi mau onse otuluka pakamwa pa Yehova . ” Conco , sitifunikanso kuyopa kupemphela mokweza poganiza kuti iye akhoza kutimvela . Ndithudi , kukonzekela kumacititsa kuti kulambila kwathu kwa pabanja kukhale kopindulitsa . Aphunzitseni m’njila yokondweletsa komanso yolimbikitsa cikhulupililo . Fotokozani kusiyana pakati pa abusa oona acikhristu ndi anthu amene amadzicha kuti ndi abusa . 15 Iwo anapulumuka cifukwa anali kuopa Mulungu ndipo anacita cifunilo cake . Kodi inu mungacite ciani ngati mnzanu wacita colakwa cacikulu kapena chimo lalikulu ? Mumtima mwake iye anati , ‘ Ngati ningafune kuloŵa cipembedzo , ningayambe ku Mboni . ’ Kuyambila nthawiyo , abale odzozedwa anayamba kukhala m’Bungwe Lolamulila popanda kutumikilanso monga otsogolela bungwe la Society . Mayankho a mafunso amenewo adzatithandiza kudziŵa mmene tiyenela kuonela kulambila mu tuakacisi . Adzatithandizanso kudziŵa kulambila kumene kumakondweletsa Mulungu . Magazini ya Watch Tower ya December 1 , 1924 inakamba kuti : “ Tikukhulupilila kuti wailesi ndiyo njila yochipa komanso yogwila mtima kwambili polengeza uthenga wa coonadi . ” Iye angasangalale ngati mutataya mwayi wokalandila moyo wosatha mwa kukana ulamulilo wa Yehova na kukhala kumbali yake . 17 “ Ndani Ali Kumbali ya Yehova ? ” Ndipo zolemba zina za m’nthawi imeneyo zikalipo . Cifukwa cosamukasamuka , Sara ndi anchito ake sanali kuphikila mkate wao mu mauvuni amene anali kugwilitsila nchito kwao ku Uri . Fotokozani cifukwa cake tiyenela kucita khama kuphunzila Baibulo . Titakumana , tinakondwela kwambili . TSAMBA 3 Cina cimene cipangitsa Yehova kukhala woyenela kulamulila n’cakuti ali na cidziŵitso ndi nzelu zom’thandiza kusamalila bwino cilengedwe . Kodi a Mboni za Yehova Amakhulupilila Yesu ? Matupi athu ndi ofanana ndi a nyama m’mbali zambili . Mau a mtumwiyo amatitsimikizila kuti olo tikumane na mayeselo yabwanji , Yehova adzatithandiza ngati timudalila . ( Sal . N’naonadi kuti maulosi amenewa anali kukwanilitsika . Kodi Mulungu akanacita ciani kuti athetse nkhani zimenezo ? Zonsezi zimathandiza anthu a Yehova kukhala ogwilizana . — Sal . 7 : 39 ) Nawonso akazi amene amagwila nchito mwakhama pa banja amayamikila kumvela tumau tolimbikitsa tocokela kwa amuna awo . ( Miy . Mutu wina wabanja ku Japan unanena kuti mwana wao wa zaka khumi samazindikila kuti nthawi yatha , iye amafuna kuti apitilizebe . Yesu anati bwanji pankhani yokhala pa mtendele ndi abale athu ? 7 : 28 ; Sal . 31 : 5 ) Monga Tate woolowa manja , amaphunzitsa coonadi anthu amene amamuopa . Cifukwa cakuti mwa cikhulupililo anaona cina cake ca mphamvu kwambili kuposa nyanja kapena gulu la asilikali . ( Yona 3 : 10 ) Yehova anasintha maganizo ataona kuti Anineve alapa ndi kusiya njila zawo zoipa . Ngati musamalila banja , n’ciani cimene mungaphunzile pa cikhulupililo cimene Inoki anali naco ? Kuyambila mu 1931 , M’bale Diehl anatumikila mokhulupilika pa Beteli ya ku Bern , m’dziko la Switzerland . Ndi liti pamene anthu a Mulungu anakhala akapolo a Babulo Wamkulu ? Musakhumudwe ngati munthu sanaonetse cidwi pa ulendo woyamba Satana akumenya nkhondo ndi abale otsalila odzozedwa a Kristu amene akali padziko lapansi . Iye akuonjezela kuukila kwake pamene watsala ndi “ kanthawi kocepa . ” ( Chiv . Funsani Mboni za Yehova kuti zikuuzeni zimene Baibulo limanena zokhudza zocitika zamtsogolo . ( a ) Yesu atapita kumwamba , n’cosankha cofunika kwambili citi cimene atumwi okhulupilika anapanga ? NYIMBO : 61 , 22 Iye anafotokoza cifukwa cake amayamikila utumiki umenewu , anati : “ Kutumikila Yehova m’dela limene sin’nazoloŵele kwanipindulitsa m’njila zambili . Mwina zoŵelenga simuzikonda kweni - kweni . ( b ) Nanga m’nkhani yotsatila tidzakambilana ciani ? Komabe , panthawiyi Yosefe anali wokonzeka kuika Yesu m’manda mwaulemu ndi kudzidziŵikitsa kuti anali wophunzila wa Khristu , mosasamala kanthu za mavuto amene akanakumana nawo cifukwa cocita zimenezo . 5 : 1 , 2 ) Ifenso tikamatumikila modzipeleka masiku ano , anthu ena ‘ adzatamanda Yehova . ’ Conco , atalephela kundiyankha , anati : “ Sindingakusinthe maganizo , ndipo iwenso sungandisinthe . . . . ( 1 Yohane 4 : 2 , 3 ) Apa n’zoonekelatu kuti Yohane anatanthauza kuti okana Kristu ndi anthu amene mwadala amafalitsa mabodza acipembedzo onena za Yesu Kristu ndi ziphunzitso zake . Yotsatila pambuyo ni hosi yofiila monga moto , ndipo wokwelapo wake akucotsa mtendele padziko lonse . Panalibenso amene akanatenga dzina la banja ndi kulandila coloŵa . Akatswili a zaumoyo amakamba kuti kucitila ena cifundo kungathandize munthu kukhala wathanzi , ndi kukhala na mabwenzi abwino . 6 : 13 ; 1 Yoh . 5 : 19 . Ngakhale n’telo , ndimapemphelanso kuti aja amene amatithandiza athe kulimbana ndi mavuto a zacuma . ” Nthawi yomweyo anthuwo anacoka kumbali zonse za mahema a Kora , Datani ndi Abiramu . Komabe , sikuti onse amene amachulidwa m’Baibulo kuti nduna anali ofulidwa . Pasanapite nthawi itali , zimene zinacitika zionetsa kuti nkhawa ya Abulahamu inali yomveka . Gulu limene nimagwila nalo nchito yomanga lili ngati banja langa . TSAMBA 23 • NYIMBO : 120 , 44 Mulungu afuna kuti anthu a mitundu yonse adziŵe coonadi molondola ndi kuti adzasangalale ndi moyo wosatha . Iye anati : “ Ndimakonda kuceza ndi anthu amisinkhu yosiyanasiyana . ” 2 : 16 , 17 ) N’zolimbikitsa kwambili kudziŵa kuti Yehova amatikonda ndi kutisamalila cifukwa ca kukoma mtima kwake . Iye anasangalala kwambili pamene atate wake anamugwila paphewa mwaphamvu ndi kumuthandiza kuti asamile . ( Miy . 6 : 16 , 17 ) Kunyada na kudzikweza kumalepheletsa munthu kukhala pa ubwenzi na Mulungu . ( Sal . Anthu adzakhala angwilo pang’ono ndi pang’ono . Mngeloyo anatsimikizila Hagara kuti : “ Yehova wamva kulila kwako . ” Pali kusiyana kwakukulu pakati pa ulamulilo wacikondi wa Yesu ndi ulamulilo wa anthu . Pofuna kuti akhale na ufulu wolalikila , iwo anakamba ndi kupambana milandu yambili ku makhoti . Patapita cabe miyezi 6 , n’nakhazikitsa maphunzilo a Baibo 17 , ndipo ena anakhala Mboni . Kodi mumakhulupilila kuti Yehova nthawi zonse amacita zinthu zoyenela ndi zacilungamo ? Woyamba ndi wakuti “ Yehova amadziŵa anthu ake , ” ndipo waciŵili ndi wakuti “ Aliyense wochula dzina la Yehova aleke kucita zosalungama . ” Pokhala opanda ungwilo , tonse timapatsidwa uphungu wa m’Malemba nthawi zina . Patapita zaka , nayenso Mfumu Hezekiya anakhala na mtima wodzikuza , koma anasintha mwamsanga . — 2 Mbiri 26 : 16 ; 32 : 25 , 26 . Cifukwa tsiku limene udzadya , udzafa ndithu . ” ( Gen . Iwo amaphunzila Baibulo ndipo adzakuuzani zinthu zabwino zimene Mulungu walonjeza kuti adzacita mtsogolo . [ Bokosi papeji 6 ] 15 “ Yehova Mulungu Wathu Ndi Yehova Mmodzi ” 53 : 2 , 7 ) N’naphunzila kuti wotsatila weni - weni wa Yesu , “ ayenela kukhala wodekha kwa onse . ” — 2 Tim . Zinthu zimene unazimva kwa ine ndi kwa mboni zambili zokhudza ine , zimenezo uziphunzitse kwa anthu okhulupilika amene nawonso , adzakhala oyenelela bwino kuphunzitsa ena . ” Nditangokamba kuti ‘ Ame , ’ foni yanga inalila . Baibulo limati : “ Wodala ndi munthu woopa Yehova , munthu amene amasangalala kwambili ndi malamulo ake . ( Ŵelengani Malaki 1 : 12 , 13 . ) Olo kuti aseŵenzetse njila yofanana , zimene amapeza zimasiyana . Mukusangalala pogwila nchitoyo cifukwa cakuti oyang’anila nchitoyo ndi acikondi . “ Adzapukuta misozi yonse m’maso mwawo , ndipo imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . 146 : 9 . 7 “ Tizisonyezana Cikondi Ceni - ceni m’Zocita Zathu ” Pakuti monga tilili ndi ziwalo zambili m’thupi limodzi , koma ziwalozo sizigwila nchito yofanana , momwemonso ifeyo , ngakhale kuti ndife ambili , tili thupi limodzi mwa Khiristu . ” — Aroma 12 : 3 - 5 . 14 Musamaone Cabe Maonekedwe a Munthu Kumadela ena , kucita zimenezo kunali kuika moyo wa munthu pa ciopsezo . Sitikukaikila zakuti imfa ndi mdani . Baibo imatiuza kuti : “ Zolingalila sizikwanilitsidwa ngati anthu sakambilana moona mtima , koma aphungu akaculuka zimakwanilitsidwa . ” — Miy . ( Aroma 5 : 8 ) Cikondi copanda dyela cinacititsa Mulungu kuthandiza anthu ofooka , osoŵa thandizo , ndi ocimwa . “ Timapezelapo mwayi woceza ndi ana athu tikhala paulendo m’motoka . Khalidwe lathu , kavalidwe kathu , ndi mmene timadzikonzela ziyenela kuonetsa kuti timalemekeza Mulungu amene amatiitana ku misonkhano yacikristu . Ndikagwila nchito , ena anali kundipatsa zakudya kapena zinthu zina zapanyumba . Akulu a m’maiko osiyanasiyana anagwilitsilapo nchito malangizo amenewa ndipo anaona kuti ndi othandiza . Kodi cikhulupililo ca Mkhiristu tiziciona bwanji ? Yesu anamutsimikizila kuti : “ Mlongo wako adzauka . ” Kodi Davide anacitanji atamva zimene Yehova anakamba ? 24 : 45 - 47 ; Aheb . YOSEFE anali kuyenda m’kanjila ka mkati mwandende mmene munali mdima kucokela ku nchito yakalavulagaga imene anali kugwila . Koma citamando conse cifunika kupita kwa Yehova . — Sal . Ise anthu a Mulungu timapewelatu kutengako mbali m’zandale kapena m’zinthu zokhudzana ndi cipembedzo conama . Koma ambili sitingapeweletu kutengako mbali m’zamalonda m’dziko la Satanali . Zimenezi zinam’kwiyiitsa Yehova . ( Luka 9 : 58 ) Anazindikila kufunika kophunzitsa ena kuti adzapitilize nchitoyo pambuyo pa imfa yake . ( 1 Akor . 13 : 2 ) Conco , tiyeni tipitilize kuonetsana “ cikondi ceni - ceni m’zocita zathu , ” osati na “ mau okha . ” Muziyesetsa kupewa nkhongole . Pankhani ya umphawi , kodi zinthu zidzasintha bwanji posacedwapa ? ( Sal . 23 : 5 ; 104 : 15 ) Inde , n’zofunika kuti okwatilana azisonyezana cikondi kaŵilikaŵili cifukwa zimenezo zimathandiza cikondi cao kukula . Nayenso Ann ni wokondwa ngako , cifukwa wakhala monga amayi ake auzimu a Paula . Masiku ano , zinthu n’zolingana ndi mmene zinalili m’nthawi ya mneneli Mika . Pofika pano , m’nkhani ino tagwilitsila nchito malemba amene agwidwa mau kapena osagwidwa mau ocokela m’mabuku 14 a m’Baibulo . Russell anali kukonda kudandaula ndi zocita za abale ndi alongo ena ndipo anali kuganiza kuti palibe cabwino cimene amacita . Imeneyi ni nkhani yaikulu . Akristu oyambilila anali ofunitsitsa kuthandiza ena panthawi ya mavuto . ( Agal . 5 : 22 , 23 ) Anapilila mayeselo aakulu kuposa amene analephela kupilila poyamba . Mwacitsanzo , kodi munali mbeta , koma lomba muli pabanja ? Kaya mwininyumba ayankhe kuti “ inde , ” “ iyai , ” kapena “ kaya , ” tembenukilani patsamba la mkati popanda kufotokoza ciliconse ndipo kambani kuti , “ Onani zimene Baibulo limanena . ” Kuti tiyankhe mafunso amenewa , tifunika kudziŵa mayankho a mafunso aŵili ofunika awa : N’cifukwa ciani zoipa zimacitika ? Ndipo Mulungu adzacita ciani ? Izi siziimila mankhwala azitsamba amene tingagwilitsile nchito panopa kapena m’dziko latsopano . Kuti mukafike kumeneko , mufunika kukwela basi . Zimenezi zikusonyeza kupita patsogolo kocititsa cidwi . Umbombo naonso ndi woipa . Baibulo limakamba kuti anaugula ndi “ magazi a Mwana wake weniweni . ” Zimenezi zidzatithandiza kuti tiziyamikila kwambili cikondi cosatha cimene Yehova amatisonyeza . — Afil . Kuciyambi kwa mbili ya anthu , mngelo wina anapandukila Mulungu ndipo anacititsa kuti anthu aŵili oyambilila apandukilenso Mulungu . Ngakhale kuti mwana wathu anafa pa ngozi ya ndeke , timakumbukilabe nthawi imene tinali kusangalalila pamodzi . Anthu olamulidwa ndi Aroma , kuphatikizapo anthu amene Yesu anali kuwalalikila , anali kupeleka misonkho yambili , monga wa katundu , malo , ndi wa nyumba . Tinali kusangalala ngako . Yehova anauza Mose kuti iwo ‘ anacita zinthu zowawonongetsa ’ komanso kuti ‘ anapatuka mofulumila panjila imene iye anawalamula kuyendamo . ’ Zimene zinacitikila Anita zikuonetsa kuti kutsutsidwa ndi anthu a m’banja kumayesa cikhulupililo ca Mkristu . Monga mmene Yehova anakambila , m’kupita kwa nthawi Adamu anafa . Mavesi ozungulila lemba limeneli , aonetsa kuti Paulo anali kukamba za uthenga kapena kuti colinga ca Mulungu cochulidwa m’Baibulo . N’cifukwa ciani tiyenela kukonda Mulungu ? Ndinali kudziimba mlandu wolephela kupezela ana anga zinthu zambili monga mmene makolo ena amacitila . Mobweleza - bweleza , Baibo imanena za lonjezo lakuti akufa adzauka . Akulu angakambilane ndi mipingo ya m’dziko limene kunacokela abalewo mwa kulemba kalata ndi kuitumiza ku ofesi ya nthambi ya m’dziko lawo kupitila pa jw.org . ( Salimo 55 : 22 ) Kodi mumakhulupilila kuti pemphelo limathandizadi ? Mkati mwa nthawi imeneyi m’pamene ine ndi Laurie tinakwatilana , ndipo tinali kufuna kupitiliza umoyo wathu wozungulila dziko . ( a ) Kodi Bungwe Lolamulila masiku ano limalimbikitsa bwanji gulu la abale a pa dziko lonse ? Ndiyeno Mulungu anati : ‘ Ndiwaononga . ’ A Zulu : Zikomo , mwaŵelenga bwino . Akhristu oona amakondanso ngakhale adani awo . — Mat . Mfundo imeneyi imatilimbikitsa kupezeka pamisonkhano nthawi zonse . 2 : 24 ) Colinga cake cinali cakuti anthu aculuke , adzaze dziko lapansi , ayang’anile nsomba , mbalame , ndi zamoyo zonse . Tikukhala ‘ m’nthawi yapadela komanso yovuta , ’ ndipo Akristu ambili okhulupilika akupilila ziyeso ndi zizunzo . Mungafunsenso apainiya kapena oyang’anila oyendela cifukwa cake io anasankha kuyamba utumiki wa nthawi zonse . Kodi izi ziyenela kukucititsa kuganiza kuti simunacite bwino kudzipeleka ? Tikacita conco , tidzaonetsa kuti timakonda ndi kuyamikila cuma camtengo wapatali cimeneci . Mwacitsanzo , Jack , amene amakhala ku United States , anagulitsa nyumba yake yaikulu na bizinesi n’colinga cakuti akhale na nthawi yocita upainiya pamodzi na mkazi wake . Nanga tingacite ciani kuti maso athu akhalebe pa iye pamene takumana na mavuto aakulu mu umoyo wathu ? Iye anawauza kuti : ‘ Malemba amati , “ Nyumba yanga idzachedwa nyumba yopemphelelamo , ” koma inu mukuisandutsa phanga la acifwamba . ’ ” — Mat . Zimenezi zinacititsa kuti kumwamba kukhale cisangalalo cacikulu koma padziko lapansi panakhala mavuto ambili kuposa kale lonse . Tilibe ufulu wonse umene Yehova ali nawo . Anthu ambili amene poyamba anali na makhalidwe monga a nyama , anasintha na kukhala a khalidwe labwino . Izi zinacititsa kuti anthu onse azimva zimene tinali kuphunzila . Kodi Yehosafati anaphunzilapo kanthu pa zimene zinacitikazo ? Ngati Yehova amathandiza mbalame kumanga zisa , ndiye kuti adzatithandiza kupeza malo oti tikhalemo pamodzi ndi banja lathu . Izi zacititsa kuti kukhale paradaiso wauzimu wa padziko lapansi umene uli na nzika zoposa 8 miliyoni . Koma popeza kuti timam’khulupilila ndi kum’konda , nthawi zonse timapempha thandizo kwa iye , ndipo timayesetsa kucita zimene tingathe kuti tidziŵe zimene iye amafuna tisanasankhe zocita . Ngati makolo amakwanitsa kuphika , kuyeletsa , kumwa mankhwala , ndi kulankhulana bwino ndi ana ao , ana sangafunikile kulamulila makolo ao pa kalikonse . ( 2 Akorinto 4 : 4 ) Satana ndiye amalamulila magulu andale ndi ofalitsa nkhani , ndipo amawaseŵenzetsa kuti aletse nchito yolalikila uthenga wabwino . Ngakhale Yesu anaona kuti kupempha Atate wake kuti am’thandize kusankha zinthu mwanzelu n’kofunika . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Cikondi . . . sicisamala zofuna zake zokha . ” — 1 Akorinto 13 : 4 , 5 . ( Mateyu 28 : 19 , 20 ) Ndinali kuopa kuti mwina ndingakumane ndi munthu amene ndinamucitila zinthu zoipa kapena kumulakwila nthawi yakale . Cikhulupililo si khalidwe limene anthu ocimwa amabadwa nalo , ndipo silibwela lokha . Zidzakhala zosangalatsa kwambili kugwilila nchito pamodzi mu ulamulilo wa Kristu , ndipo m’kupita kwa nthawi , tonse tidzakhala angwilo . Koma anaopa kuti Akhristu aciyuda odulidwa a mumpingo wa ku Yerusalemu adzaleka kumulemekeza akaona kuti akuyanjana ndi Akhristu amitundu ina . ( Aef . 4 : 2 ) Onani kuti pamenepa , Paulo sanakambe cabe kuti ‘ tizilolelana . ’ Tifunika kukoka mpweya wokwanila . Abale athu akakumana ndi mavuto , tiyenela kuwatonthoza ndiponso kuwapatsa thandizo lofunikila lakuthupi ndi lakuuzimu . ( Miy . Gulu la Yehova limayesetsa kumanga Nyumba za Ufumu ndi kupeleka ndalama zothandiza pa nchito yomanga nyumbazi . Posapita nthawi , ndinasintha mmene ndinali kuonela zinthu ndipo ndinayamba kutumikila Yehova mosangalala . Zinali zovuta kwambili kuti amai avomele kupita kunyumba yosungila okalamba . ( b ) Nanga zoyesa - yesa zawo zakhala na zotulukapo zanji ? 4 Yehova Amatitonthoza m’Masautso Athu Onse Imati anali mu “ ukapolo wa mtundu uliwonse umene anatha kuwagwilitsa nchito mwankhanza . ” 7 : 17 - 24 . Nili na gulu la anthu ogontha pa msonkhano wacigawo ku Cleveland , Ohio , mu 1946 ( Mat . 5 : 23 , 24 ) Mulungu adzatidalitsa ngati timakonda abale athu ndi kuyesetsa kukhala pa mtendele ndi io . Conco , cinthu cofunika kwambili cimene mungacite kwa wofedwa ndi kumumvetsela popanda kum’dula mau . ” Anamuphunzitsa kukonda Yehova na Mau ake . Anagwilitsila nchito zikwangwani , manyuzipepala , ndi tumapepala toitanila anthu tokwanila 710,000 . Mwacitsanzo , Baibo imakamba kuti mmodzi wa Akhristu odzozedwa a m’zaka 100 zoyambilila anacotsedwa mumpingo . Koma pambuyo pake anabwezeletsedwa . ( 1 Akor . 5 : 1 - 5 ; 2 Akor . Monga mwa kunena kwa Malemba , kudzicepetsa ndiko njila yanzelu nthawi zonse . Mfundo imeneyi iyenela kutipangitsa kukhala osangalala mosasamala kanthu kuti tinaphunzila coonadi m’njila yotani . Pa zifukwa zimenezi , kudzicepetsa n’kofunikabe kwa anthu onse a Mulungu , ndipo Yehova amakonda ngako anthu odzicepetsa . Tikukhala ‘ m’nthawi yapadela komanso yovuta . ’ M’bale ndi mlongoyo anaonetsa Khalidwe Lopambana . 19 , 20 . Ciliconse ca m’dziko lapansi cidzafa . ” ( Ŵelengani Machitidwe 6 : 1 . ) Kodi Mulungu amasangalala ndi anthu amene amapanga ulendo wautali wopita ku tuakacisi kukalambila ? ( Mat . 13 : 34 ) Mafanizo amagwila mtima , ndipo mfundo zake zimakhudza mtima mosavuta . ( b ) Nanga zimenezo zinawakhudza bwanji ophunzila a Yesu ? Koma pomalizila pake anaonekela kwa ine , ngati khanda lobadwa masiku asanakwane . ” — 1 Akor . Mmodzi mwa anthu amenewa anali mkulu wa asilikali , amene anali ndi udindo wapamwamba kwambili m’dzikolo kuposa onse kupatulako pulezidenti yekha . Ngati ndife odzicepetsadi , tidzapewanso kuganiza kuti ndife oposa anzathu . ( Rom . Conco , anapempha mzimayiyo kuti amudziŵitse dzina na adresi yake . Ena amafunsila malangizo kwa okhulupilila zakuthambo , ndipo kaŵili - kaŵili nkhani zawo zimapezeka m’magazini na m’manyuzipepa . Adolfo amati ni wokondwela kwambili ndi mmene wasinthila umoyo wake . Nthawi yolengeza uthenga umenewu idzakhala itatha , ndipo nthawi ya “ mapeto ” idzakhala itafika . ( Mat . N’cifukwa ciani anatelo ? ( The Book — A History of the Bible ) Macaputala amene ali m’Baibulo masiku ano , ndi Langton amene anawagaŵa . M’Baibo , Salimo 37 imapeleka yankho na citsogozo kwa ise masiku ano . Yefita anadziŵa kuti afunikila thandizo la Yehova kuti akwanitse kulanditsa Aisiraeli kwa Aamoni . ( Afilipi 4 : 8 ) Tikamalalikila timalimbitsa cikhulupililo cathu cifukwa cakuti timakumbukila malonjezo a Mulungu ndi mfundo zake zabwino . Kukamba zoona , Baibulo ndi buku losavuta kumvetsa . Pamene tinadzipeleka kwa Yehova , tinalonjeza kuti tidzacita cifunilo cake zivute zitani . N’cifukwa ciani Paulo anakamba mosapita m’mbali polembela Akristu aciheberi ? “ Ndimasinkhasinkha zikumbutso zanu . ” — SAL . Komanso , popeza kuti zipangizo zamakono n’zofala , mwina mumakonda kumvetsela nyimbo zabwino zoimbiwa na akatswili . 24 : 15 ) Tidzakhala na nchito zambili zokondweletsa , zimenenso zidzapangitsa kuti Yehova atamandike . Conco ndinaganiza kuti ndinali woipa kwambili ndipo Mulungu sakanatha kundithandiza . ” Kodi pamenepa Yesu anali kukamba zinthu ziti ? Poyamba , ine ndi Amai tinali kukonda kukambitsilana zimene ndaphunzila . INE n’nakulila ku Graz , m’dziko la Austria . ( Maliko 10 : 29 , 30 ) Utumiki wao pa Beteli umawapatsa mpata wosonkhana ndi kutengako mbali mu ulaliki mlungu uliwonse . 17 : 6 ; Yak . Kale , mneneli Yesaya anauzilidwa kulemba mmene zinthu zidzakhalila m’Paradaiso wolonjezedwa . Kuonjezela apo , tili ndi ciyembekezo cabwino ca mtsogolo . M’nkhani ino , tikambilana maganizo amene tiyenela kupewa , ndiponso mmene tingapindulile ndi cakudya cakuuzimu cimene Yehova amatipatsa . Anthu ambili amakonda kumvetsela nyimbo ndi zinthu zina poyenda , powacha , kapena pocita zinthu zina . Tinali kupita mu ulaliki na kucititsa misonkhano . 3 : 12 , 13 ) Conco , nthawi ndi nthawi tiyenela kupenda colinga cathu potumikila Yehova . Mose anakumbutsa Aisiraeli kuti Yehova sadzasintha , ndipo adzapitiliza kuwakonda ndi kuwasamalila . Anthu ambili amalila munthu amene amamukonda akamwalila . Cinsinsi Namba 12 Zolinga 4 : 2 , 3 . Pemphani Yehova kuti akuthandizeni kuseŵenzetsa zimene mwaphunzila m’Mau ake . Mzimu wa Mulungu unatsogolela Yesu kucipululu . Iye anakamba kuti : “ Baibulo landithandiza kukhala ndi umoyo waphindu ndi kukhala ndi ciyembekezo cabwino ca mtsogolo . Iye anati , “ Ndimaona kuti mwamuna wanga amandikondadi , ndipo ndimazimva kuti ndine woyandikana naye . ” Ganizilani fanizo limene Yesu anakamba pa Mateyu 18 : 23 - 34 . Tingapindule na uthenga wa m’Baibo maka - maka ngati imapezeka m’citundu cimene timamvetsetsa . Komanso amafuna kukhala mwamtendele ndi ena . Dziko lidzakhala losangalatsa pambuyo pakuti Mulungu waononga oipa onse . 5 : 28 , 29 . M’bale amene wapeleka nkhani ya cikwati cao akuona okwatilanawo agwilana manja mwacikondi , ndipo akuganiza kuti , ‘ Kodi cikondi ca aŵiliwa cidzapitiliza kukula pamene zaka zikupita ? Komanso , Mariya ‘ anasunga mosamala kwambili mawu onsewo mumtima mwake . ’ Limeneli linali Baibulo loyambilila kumasulidwa , ndipo linali limodzi mwa Mabaibulo ofunika kwambili . ( Mat . 6 : 24 ) Ngati tiika patsogolo nchito yotumikila Yehova na kuphunzitsa ena Mau ake , tidzakhala na cimwemwe coculuka . Nkhani ziŵilizi zidzayankha mafunso amenewa , ndipo zidzatithandiza kucilimika polimbana na Mdyelekezi . Ena amakumbukila ndi kulakalaka nthawi imene anali kugwila nchito mu kafiteliya . Kudziŵa mayankho a mafunso amenewa kungatithandize kudziŵa ngati Akhristu ayenela kukondwelela Khrisimasi kapena ayi . ZA MKATI : Lili ndi mabuku 39 olembedwa m’Ciheberi ( mbali zina zocepa zinalembedwa m’Ciaramu ) ndipo ena 27 analembedwa m’Cigiriki 7 : 11 , 21 , 24 , 25 ) Umbombo wafala ndipo ungasoceletse aliyense . ( Genesis 1 : 28 ; Yobu 38 : 4 , 7 ) Mwacitsanzo , ganizilani anthu amene Yesu anaukitsa . Akakhopela kapena kuyang’ana kacizindikilo kena zimakhala ngati wadiniza pa mausi ya kompyuta . Afunseni kuti ni nchito iti imene apainiya angacite . 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani nkhani ya ukapolo na ufulu inali mkamwa - mkamwa m’nthawi ya mtumwi Paulo ? Iye anayamba kuphunzila Baibulo na Mboni za Yehova . Ndipo m’caka ca 2000 , anakhala wa Mboni za Yehova . Nanga n’ciani cimacitika Mkristu wobatizidwa akacita chimo lalikulu cifukwa ca kufooka ? ( Mac . 2 : 42 ) Atumwi ndiwo anali kuyang’anila ndalama za mpingo . ( Aroma 16 : 3 - 7 , 13 ) Mwacitsanzo , Paulo anavomeleza kuti Anduroniko ndi Yuniya anatumikila Kristu kwa nthawi yaitali kuposa iye . Iyai sitingatelo . Koma tingacite bwino kuona ngati Yehova waticilikiza m’njila imene sitinazindikile . Hana anali kulila nthawi zambili cifukwa comatonzedwa na mkazi mnzake Penina . Baibo siinakambe . 4 : 34 , 35 ) Pambuyo pake , mumpingo munabuka vuto lalikulu . Malemba samakamba zambili ponena za maonekedwe a Yesu . 29 : 5 , 7 ) Amene anasunga mau a Mulungu anakhala umoyo wabwinoko ku Babulo . Wolankhulila Mulungu analosela kuti : “ Mwana wamwamuna adzabadwa m’nyumba ya Davide , dzina lake Yosiya . . . Mwacitsanzo , mdzukulu wa Nowa , Nimurodi , anatsutsa kwambili ulamulilo wa Yehova . * Mofanana ndi Akhristu ena obatizika , iye adzapitiliza kuwonjezela cidziŵitso cake pa colinga ca Yehova . 119 : 97 . 5 : 9 ) Kulibenso kwina kumene tingapeze cikondi ngati cimene cili pakati pa anthu a Mulungu . Mwacitsanzo , Aisiraeli atapulumutsidwa kwa Farao ndi magulu ake ankhondo pa Nyanja Yofiila , io anaonetsa cisangalalo cao mwa kuimba nyimbo zacitamando ndi ciyamiko zogwila mtima . ( Eks . Kwa zaka zambili , ndinali kupita kumanda pafupifupi tsiku lililonse . Awa ndi mau amene anthu ena amakamba akaona ana ofanana kwambili ndi makolo ao . 2 : 4 - 6 ; Yoh . 1 : 29 . Palibe cifukwa cofuna kudziŵila kuti ndani analandila matalente asanu kapena ndani analandila aŵili . Ngakhale kuti sitingapite kumalo osoŵa , tikhoza kupeza njila zatsopano zimene tingalalikilile . Pokamba za lonjezo la Mulungu kwa Danieli , Baibo yochedwa Jerusalem Bible imati : “ Udzauka kuti ulandile gawo lako kumapeto kwa nthawiyo . ” Iye anakamba kuti ulamulilo wake ndiwo wabwino kuposa wa Mulungu . De la Fuente ) , Na . M’kupita kwa nthawi , anayamba kunitumiza kukayendela nthambi za ku maiko ena . Mwacitsanzo , mu November 2013 , cimphepo camphamvu camkuntho cochedwa Haiyan , cinasakaza cigawo capakati ca dziko la Philippines . Cimphepoco cinawononga nyumba za mabanja opitilila 1,000 a Mboni . Ndipo akuluwo akapeza kuti sanaphe mnzake mwadala , munthuyo anali kufunika kukhala mumzinda wothaŵilako mpaka mkulu wa ansembe atamwalila . M’kukambilana kwawo , mlongoyo anazindikila kuti nkhani imene inam’khumudwitsa sanaimvetsetse , ndiponso siinali kukhudza Janet . Pamene Akhristu a m’zaka 100 zoyambilila ku Yudeya anakhudzidwa na njala , Akhristu anzawo anawathandiza . Zimenezi n’zosadabwitsa cifukwa cakuti io si odzozedwa . “ Tifunika kudziŵa colinga ca moyo ” Koma m’zaka ziŵilizo , mkaziyo anagwilizana na abale na alongo ena , ndipo nawonso anakhala mabwenzi ake apamtima . Mwina boma lingalamule kuti ngati anthu asonkhana kuti alambile Yehova , ayenela kulipila ndalama , kumangidwa , kapena kupatsidwa cilango cina cacikulu . 3 : 10 ) Okwatilana akavala “ cifundo cacikulu , kukoma mtima , kudzicepetsa , kufatsa , ndi kuleza mtima , ” amakhala osangalala ndipo amateteza cikwati cao . Kodi mbadwa za Adamu ndi Hava zinakhudzidwa ndi zimene makolo ao anacita ? lonjezo la kudzipeleka kwanu kwa Mulungu ? Kumbukilani kuti anthu amene amayambitsa ndi kufalitsa mabodza amenewa amakondweletsa Satana Mdyelekezi , “ tate wake wa bodza . ” Atangofika kumeneko anapeza anthu amene anali kufuna kuphunzila coonadi ca m’Baibulo . Pa Aroma 6 : 7 pamati : “ Munthu amene wafa wamasuka ku ucimo wake . ” ( a ) N’cifukwa ciani kupemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele n’kofunikabe ? 5 : 1 ) Izi zitanthauza kuti iwo amayesetsa kuphunzila mmene Yehova amaonela zinthu , ndipo amayamba kuziona mmene iye amazionela . CIPILALA CIMENECI CIMALEMEKEZA TITO AMENE ANALI MMODZI WA MAFUMU OCHUKA A ULAMULILO WACIROMA . 1 : 4 ) M’zaka zaposacedwapa , kusintha kumeneku kwakhala cinthu covuta kucilandila kwa Akhiristu ena . Caputa 24 ca Machitidwe , cifotokoza za Paulo pamene anapita kukaonekela kwa bwanamkubwa waciroma , Felike . ( 1 Akor . 7 : 39 ) Tonse tidzaŵelengeledwa mlandu kwa Mulungu . Mfundo imeneyi iyenela kukumbutsa onse ali m’vikwati kuyesetsa kumathetsa msanga mavuto madzi akali m’nkhongono . Yehova angacititsenso cilengedwe cake kucita zimene iye afuna . ( Chiv . 20 : 6 ) Mulungu wawapatsadi ciyembekezo cabwino kwambili . N’zoona kuti pa mlingo wina wake , iwo amakhala ataphunzila kale kudzilanga okha . Kodi mphatso ya mtengo wapatali imeneyi inam’cititsa kumva bwanji Shannon ponena za Yehova ? 30 Zimene Mungacite Kuti Kuŵelenga Baibo Kwanu Kukhale Kopindulitsa Komanso Kokondweletsa Ngati ticitila zabwino anthu ena , timacepetsako nkhawa zathu . Kodi mfundo imeneyi ni ya zoona ? ( a ) Kodi nchito yakuthupi tiyenela kuiona bwanji ? Ndili ndi zaka 15 , ndinacotsedwa pa sukulu yophunzitsa cikhalidwe ndipo ndinasowa kokhala . ( Mat . 28 : 19 , 20 ) Ngati colinga canu ni kupanga ophunzila , ndiye kuti mwasankha nchito yabwino kwambili imene idzakuthandizani kulemekeza Mulungu . Nanga n’ciani cinam’thandiza kupilila ? Masiku ano , alambili a Mulungu ofika m’mamiliyoni , amatsatila citsanzo ca Yesu . Iwo amasumika maganizo pa ciyembekezo cawo , ndipo salola kuti mayeselo awafooketse . N’cifukwa ciani masiku ano sitiyembekezela kuti Mulungu adzaticilitsa mozizwitsa ? 14 : 1 , 4 . Mu 607 B.C.E . , Ababulo anagonjetsa mafuko aŵili a ufumu wa Yuda wakumwela ndi kutenga anthu kupita nawo ku Babulo . Pambuyo pake , anthu ena anacita cidwi ndi coonadi ndipo anabatizidwa . ( Aroma 6 : 23 ; 8 : 2 ) Ndithudi ! Ndipo popeleka nsembe iliyonse , Aisiraeli anafunikila kutsatila malangizo oikidwa . Iye ndiye amaika cizindikilo onse amene adzapulumuka Ifenso timakhulupilila kuti tikafunafuna Ufumu coyamba , Yehova adzasamalila zosoŵa zathu zakuthupi . — Mat . N’zotheka kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova . Iye anali atangolimbikitsa kumene Akhristu ‘ kuwongola njila zimene mapazi awo anali kuyendamo . ’ Ndiponso , ngati mumpingo mwanu muli munthu amene anacita masinthidwe aakulu mu umoyo wake kuti ayambe kutumikila Yehova , mungam’pemphe kuti adzakusimbilenkoni cimene cinam’thandiza kusintha . Tingamutamande ndi kumuyamikilanso cifukwa ca zinthu zimene amaticitila . Mfumuyo iyenela kuti inali yokonzeka kutsatila malangizo a Natani amene anali mnzake komanso munthu amene anali ndi mzimu wa Yehova . — 2 Sam . Kodi nyambo ina imene Satana amaseŵenzetsa ni iti ? Nanga tingaipewe bwanji ? Akadzaononga adani a Mulungu , Mfumu Mesiya adzaponya Satana ndi ziŵanda zake kuphompho kwa zaka 1,000 . ( Chiv . Ngati n’conco , ndiye kuti munataya mwayi wa maceza okondweletsa ndi wopeza mabwenzi okhalitsa . Pulofesa W . 12 : 9 ) Mwa kucita zimenezo , Satana anatsutsa kuti Mulungu ndiye woyenela kulamulila cilengedwe cake . Nthawi zina Mkhiristu angakhale ndi mwamuna kapena mkazi amene si Mboni . Musazengeleze kuonana ndi Mboni za Yehova kapena kuŵelenga nkhani za pa webusaiti yawo ya jw.org . ‘ Mvelani ndi Kumvetsa Tanthauzo Lake ’ Si capafupi kulamulila mkwiyo ngati wina watikhumudwitsa kapena waticitila zinthu zopanda cilungamo . Koma ngati mwaona kuti mufunika kusintha zinthu zina pa umoyo wanu kuti muziika zinthu za Ufumu patsogolo , ndiye kuti Yehova wakuuzani zimene mufunika kuongolela kuti mulimbitse ubwenzi wanu ndi iye . — Mat . Ndi liti pamene pangano la Yehova ndi Abulahamu linayamba kugwila nchito ? M’malomwake , anaikamo maina audindo monga akuti “ Mulungu ” kapena “ Ambuye . ” Komabe m’Baibulo , maina audindo amenewa sagwilitsidwa nchito ponena za Mlengi cabe , koma amagwilitsidwanso nchito ponena za anthu , mafano , ngakhale Mdyelekezi amene . — Yohane 10 : 34 , 35 ; 1 Akorinto 8 : 5 , 6 ; 2 Akorinto 4 : 4 . Pamati : “ M’masiku a mafumu amenewo , Mulungu wakumwamba adzakhazikitsa Ufumu umene sudzaonongedwa ku nthawi zonse . ( Yes . 2 : 2 , 3 ) Mofananamo , mneneli Zekariya anakambilatu kuti “ anthu ambili a mitundu ina ndiponso mitundu yamphamvu ya anthu idzabweladi kudzafunafuna Yehova wa makamu mu Yerusalemu . ” N’ciani cimene vinyo wa pa Cikumbutso umaimila ? Iye ndiye Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi . ” Cilamulo cimeneco cinawateteza ku khalidwe loipa ndi kuwathandiza kukhala ndi mabanja acimwemwe ndi mabwenzi abwino . Kodi mungatengele bwanji citsanzo ca Hezekiya potumikila Mulungu ? Mwininyumbayo anali kulandila thandizo la mankhwala a kansa ndipo anali kukhala cabe m’nyumba . N’ndani maka - maka amene ali na udindo wophunzitsa ana coonadi ? Yesani kuganizilako njila zina . Caka cisanathe , kunakonzedwanso msonkhano wina , ndipo M’bale Frederick Franz wocokela ku likulu anaticezela . 4 : 9 , 10 ) Cifukwa ca cikondi ca Mulungu , tikhoza kukhululukidwa macimo , kukhala na ciyembekezo , ndi kudzapeza moyo wosatha . ( 2 Tim . 2 : 16 - 18 ) Komabe , Yehova sanangoyang’ana cabe . Ndipo Paulo ayenela kuti anadziŵa bwino zimenezi cifukwa ca mmene Mulungu anacitila ndi Kora ndi anthu ake patapita zaka mahandiledi . Kodi m’bale wina anali kuliona bwanji gulu la Mulungu looneka ? Koma ife timayamikila Yehova cifukwa cakuti watithandiza kukhala pamtendele ndi kumvetsetsa coonadi . Akatswili ena amanena kuti zimenezi zimacitika cifukwa ca khungu la mtundu winawake limene limacititsa munthu kusaona kapena kuiŵala cinacake cifukwa cokhala wotangwanika . Ndi lotonthoza kwambili . Mulungu amafuna kuti muzicita umutu wanu mwacikondi , monga mmene Yesu amacitila . Kodi simungavomeleze kuti nchito yathu yolalikila uthenga wabwino ni yaikulu komanso yopindulitsa ? — Mat . Lomba nimalalikila m’mudzi mwathu . Koma pamene thanzi yanga inali bwino n’nali kupitanso kukalalikila ku gawo lopanda ofalitsa , limene lili pa mtunda wa makilomita 160 . Ngakhale n’conco , akulu angaphunzile zambili mwakuona mmene Samueli anacitila zinthu ndi Sauli . ya April 2009 muli nkhani yakuti , “ Zimene Acinyamata Amadzifunsa . . . “ Ndinali kuphunzila mphindi 15 kapena 30 mwinanso kuposapo malinga ndi nthawi imene ndinali nayo . ” — Viniana , Australia . Yehova watipatsa ‘ lamulo langwilo , ’ limene limatiuza zonse zimene tiyenela kucita . M’fanizo la wofesa mbewu , mbewu ikuimila “ mau a Mulungu , ” kapena kuti uthenga wabwino wa Ufumu . Kodi Yehova watisungila ciani mtsogolo ? ( Mat . 24 : 14 ) Mapulogilamu a pa zipangizo za makono amene timaseŵenzetsa mu ulaliki , amakonzedwanso nthawi na nthawi . Pikica iyi ikuonetsa mmene zimakhalila pamene abale akuphunzitsa Baibo akaidi acidwi m’ndende za ku Bulgaria . Nanga n’cifukwa ciani ? Makolo ena amene atumikila mumpingo wa cinenelo cina , azindikila kuti ana awo sakonda kwambili coonadi . Komanso , nthawi ina mkazi wa Potifara ananamizila Yosefe kuti anafuna kum’gwilila , ndipo anaponyedwa m’ndende . Dziŵani kuti Mulungu sangawagwilitse mwala anthu amene amayembekezela pa iye . — Mat . ( Maliko 8 : 15 ) Pamene Yesu anakamba kuti cofufumitsa ca Herode , zionetsa kuti anali kukamba za a cipani ca Herode . tizidziona moyenela ? Kodi Yehova amaziona bwanji nchito zacifundo zimene timacitila anthu ena ? YELEKEZELANI kuti mukuyenda mu mseu m’madzulo ndipo kuli mdima . Palembali timapezapo mau a Yesaya akuti : “ Ndani anayezapo mzimu wa Yehova ? Ndi munthu uti amene angamupatse malangizo kapena kumuphunzitsa kanthu ? ” Kupita patsogolo kwa luso la zopangapanga kwacititsa anthu kuganiza kuti akhoza kuthetsa mavuto . Ciphunzitso cimeneci cinali cofala kwa zaka mahandiledi ambili . ( b ) Malinga ndi 1 Akorinto 15 : 28 , kodi Yesu adzacitanji panthawi yake ? Ngati timvela Mulungu , iye adzatikonda na kutidalitsa . — Deut . Satana ndi wodzikonda ndipo sasamala za inu Zoipa za tsiku lililonse n’zokwanila pa tsikulo . ” Kodi Akristu odzozedwa okhulupilika anakanapo kuthandiza anzao ? Liu lakuti Septuagint limatanthauza “ 70 . ” Boma la Roma linapatsa Ayuda ufulu wambili . Poyamba , iye anali kucita zoyenela pamaso pa Yehova ndipo anali kufunafuna Mulungu . Ndipo kaŵilikaŵili , mau pampukutupo anali kulembedwa mbali imodzi . Koma Yehova ni “ Mulungu wacoonadi . ” ( Sal . Yehova anapempha Aisraeli kuti azikomela mtima alendo . Mwacionekele , anali kuchula dzina la Mulungu monyoza ndi mopanda ulemu . — Genesis 4 : 8 , 23 - 26 . Ngakhale pa cocitika cimeneci , Luka anagwila mau a Mariya , osati a Yosefe . Kodi zimenezo si zoona poyelekezela ndi atate auzimu , amayi , abale , alongo ndi ana amene timapeza ? Anthu okhala m’Paradaiso adzayamba kugwila nchito zokondweletsa zokha - zokha . Cifukwa cosaloŵelela m’nkhondo , masauzande a Mboni , acicepele ndi acikulile , amuna ndi akazi , amazunzidwa . Mwa mphamvu ya mzimu woyela , pang’ono m’pang’ono tingayambe kuganiza mofanana ndi Khristu . Kuwonjezela apo , ngati taona kuti pali cinacake coipa cimene cingacitike , tiyenela kucitapo kanthu mmene tingathele kuti cisacitike . N’nakhala nawo m’banja kwa zaka 55 . Iwo anali mwamuna wabwino kwambili . Kodi pemphelo linawatonthoza bwanji anthu ena ochulidwa m’Baibo ? Kodi mkangano pakati pa Eodiya na Suntuke mwina unayamba bwanji ? Nanga mavuto aconco tingawapewe bwanji ? Anayesetsa kunilimbikitsa . Kodi kucita ciwawa pofuna kuthetsa zinthu zopanda cilungamo n’koyenela kwa Akhristu ? Fotokozani . Pa kompyuta pamaonekela zithunzi zoimila mau ndi ziganizo zimene zimathandiza Jairo kulankhula ndi ena . NKHANI ya m’Baibo ya pa Genesis 22 : 6 imakamba kuti , pokonzekela ulendo wokapeleka nsembe ku malo akutali , Abulahamu “ anatenga nkhuni zokawochela nsembe zija n’kumusenzetsa Isaki mwana wake . Mau ake acifundo . 1 : 26 . Kodi inu mumakhulupilila kuti Mulungu adzakuthandizani kupeza mnzanu woyenelela amene angakukondeni ? Iwo mwanzelu amasankha anthu amene ali ndi cikhulupililo colimba kuti akhale anzao , kuti aziwathandiza ndi kuwalimbikitsa . ( Sal . 36 : 9 ) Ngati tigwilitsila nchito moyo wathu kucita cifunilo ca Mulungu , tidzadalitsidwa panopa ndi kukhala ndi ciyembekezo ca moyo wamuyaya m’dziko latsopano . ( Miy . 10 : 22 ; 2 Pet . Adzacita zimenezi cifukwa iye ndi Mulungu wacikondi ndipo amadana ndi zoipa . Mau a Mulungu amatilonjeza kuti : “ Ocita zoipa adzaphedwa . Kodi tifunika kucita ciani ngati tili na nkhawa kwambili cifukwa ca vuto linalake ? Nanga tiyenela kuyembekezela ciani ? Koma kodi izi zitanthauza kuti sitiyenela kukonda kwambili acibale athu ? M’zaka zapitazi , tinayamba kuseŵenzetsa webusaite ya jw.org na JW Broadcasting . N’cifukwa ciani gulu la Mulungu linasintha zinthu zina m’zaka zapitazi ? ( Agal . 2 : 9 ) Iye analimbikitsa Akhristu anzake mwa kuonetsa khalidwe la kulimba mtima pa Pentekosite na pambuyo pake . ( Yoh . 3 : 16 ) Ngati tili ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha padziko lapansi tiyenela kupitilizabe kutumikila Yehova mokhulupilika . Tikatelo , sitiyenela kukaikila kuti iye adzatidalitsa kwambili m’dziko latsopano . ( 2 Timoteyo 1 : 5 ) Nanga bwanji ponena za wacicepele Timoteyo ? Kodi mungaphunzile ciani kwa Yesu ? Anthu ambili m’dzikoli amaona kuti afunika kukhala okhulupilika kwambili ku dziko lao , mtundu wao , kapena cikhalidwe cao , ngakhalenso ku timu yamaseŵela ya m’dziko lao . 5 : 16 ) Tiyeni tithandize anthu ambili kulandila coonadi mwa kukambilana nao bwino . Baibulo lili ndi malangizo acindunji okhudza zosalungama zimene Akristu ayenela kuleka kapena kukana . Iye adzaima pamaso pa mafumu . Sadzaima pamaso pa anthu wamba . ” — Miyambo 22 : 29 . Timadziŵa kuti uthenga wa m’Baibulo uli ndi mphamvu kuposa mau athu . — Aheb . ( Miyambo 8 : 30 ) Atumiki a Yehova naonso anali kugwila nchito pamodzi mogwilizana . ( Yoh . 21 : 15 ) Conco tinaganiza zosamukila kumeneko . ‘ AKUONEKELA M’ZINTHU ZIMENE ANAPANGA ’ Nthawi zambili , munthu wakhungu ali ndi luso lokhoza kumva ndi kukhudza zinthu , limene limamuthandiza kudziŵa zinthu zimene sangaone . Tingathandizile bwanji kusunga ciyelo ca mpingo ? Pamene Atate anamucondelela kuti akambe ngakhale liu limodzi lokha , misozi inalengeza m’maso mwa Jairo . Monga mmene tidzaphunzilila , mafunso awa angatithandize kudziŵa zimene anthu amafuna kuti tiwacitile ndi mmene tingakambitsilane nao bwino . — 1 Akor . M’nkhani ziŵilizi , tidzaona mmene acicepele angaseŵenzetsele luso lawo la kulingalila kuti alimbitse cikhulupililo cawo na kuciteteza . Pewani kuganizila cabe za ndalama zimene mumapeza cifukwa cogwila nchitoyo . Kwa zaka zambili , cinali covuta kuti anthu atumikile Yehova monga mmene cinalili covuta kwa Aisiraeli pamene anali akapolo . ( Yes . 40 : 15 ) Mtolankhani wina anafika ponena kuti “ kungakhale kudzitukumula kukhulupilila kuti kuli Mulungu amene amacita cidwi ndi zinthu zimene timacita . ” Kodi Ayuda amene anabwelela ku Yerusalemu anakumana ndi mavuto anji ? “ Mwamuna wanga anandiuza kuti akucoka panyumba . ▪ Anali Kukonda Anthu Pali enanso amene amaganiza kuti imfa ndiye mapeto a zonse . Tsiku lina , Hana akupemphela pa kacisi , Mkulu wa Ansembe Eli anam’nena kuti waledzela . Koma Yesu anakana . Mnzanga anali atabwela ndi Mboni za Yehova ziŵili . Zimene ndifuna si zimene Yehova angaone kuti n’zimene ndifunikila . ” Greg , wa zaka 60 , watumikila ku Saipan kuyambila mu 2010 . Mwacionekele tingaganize kuti iye amatengela maganizo a anthu , monga ciphunzitso ca cisanduliko . ( Sal . Ŵelengani Maliko 5 : 25 - 34 . Iye anali kupempha Yesu mobwelezabweleza kuti akatulutse ciŵanda mwa mwana wake wamkazi . 17 : 10 . Kodi mau amene Paulo anagwilitsila nchito m’lembali ndi ofunika motani ? Iwo anali ndi anchito 17 pa kampani yao yopanga zipangizo za m’makina . Izi n’zimene zinacitika kwa atumiki a pa Beteli ambili , pamene anaphatikiza pamodzi nthambi za ku Denmark , Norway , ndi Sweden ndi kupanga ofesi ya nthambi ya Scandinavia kumpoto kwa Europe . Kukhala mlaliki wopambana sikumadalila pa kuculuka kwa zofalitsa zimene timagaŵila , maphunzilo amene timacititsa , kapena anthu amene tathandiza kukhala atumiki a Yehova . Mosasamala kanthu za ukalamba ndi “ masiku oipa , ” io apitilizabe kutamanda Mulungu mmene angathele . Iye anakamba kuti , m’bale Knorr anatsatila mosavuta mfundo zimene abale ena anazikaikila , zimene zinatuluka mu Nsanja ya Mlonda yacingelezi ya mu 1925 , pa mutu wakuti “ Kubadwa kwa Mtundu . ” Apo tikumemeza nkhani ya anthu onse pamodzi na ena m’tauni ya Rochester , ku New York , mu 1953 N’ndani anapatsa Yesu mphamvu zogonjetsa ? Komabe , tingakhale bwanji Mboni za Yehova ndi za Yesu panthawi imodzi ? Mwana wathu mmodzi yekha anali atacoka panyumba ndipo makolo athu anali atamwalila . Tinalinso ndi ndalama zocepa zimene makolo athu anasiya . Monga mwa mau awo , atate anacoka pakhomo . Iye samalonjeza aliyense kuti adzam’patsa mnzake wa m’cikwati . ( Neh . 2 : 1 - 6 ) Ngati tipitilizabe kupemphela ndi kuzindikila kuti Yehova amayankha mapemphelo athu , cikondi cathu pa iye cimakula . Zida zimenezi zinakonzedwa kuti zizitithandiza kupindula kwambili na phunzilo lathu laumwini ndi labanja . “ Pa phunzilo limeneli ndinapeza mayankho a mafunso anga onse ndi enanso ambili . ” — Bertha , Mexico . Ndithudi , ni dalitso lalikulu kwambili kukondedwa na ‘ gulu lonse la abale m’dzikoli . ’ ( 1 Pet . “ PADUTSE NTHAWI ZOKWANILA 7 ” Kodi cifukwa cake n’citi ? ( Ŵelengani Salimo 127 : 1 . ) Iwo akanafuna akanagwilitsila nchito nthawi imeneyo kuceza ndi ana komanso adzukulu ao . WOYANG’ANILA DELA : Posapita nthawi , m’bale wake wamkulu kwambili wa Davide , Eliyabu , anamva zimene Davideyo anakamba . ( b ) N’cifukwa ciani Mulungu anakana Aisiraeli ? Mwacimwemwe , iye anakambanso kuti : “ Tinayamikila kwambili cifukwa cakuti tinalandila cakudya coculuka cakuuzimu kudzela mumpingo . Mosasamala kanthu za mavuto amenewa Matthew anati : “ Kutumikila ku Russia cinali cosankha cabwino kwambili pa zosankha zonse zimene ndinapangapo . ” Yesu anauza ophunzila ake kuti ‘ akaphunzitse anthu . . . , kuti akhale ophunzila ndi kuwabatiza . ’ Caka cimodzi m’mbuyomo Yesu asanakambe zimenezi , iye anafotokoza zimene wotsatila wake aliyense afunika kucita . ( Mat . Katswili wina wa zamaphunzilo , dzina lake Joachim Jeremias , analemba kuti : “ Ngakhale kuti zimene Agripa analemba sizichula mwacindunji za maulendo opita ku Yerusalemu , mfundo ndi yakuti anthu anali kupita ku Yerusalemu cifukwa Ayuda onse acikulile anali kulamulidwa kupanga maulendo amenewa . — Deuteronomo 16 : 16 . Dziwe lakale losambilamo ku Yerusalemu Mlengi wathu anatilonjeza moyo wosatha , pano padziko lapansi . 5 : 22 , 23 ) Wamasalimo analemba kuti : “ Odala ndi anthu amene Mulungu wawo ndi Yehova . ” Ganizilani zimene Yehova akucita masiku ano na zimene imwe mungacite mu utumiki wake . Kumbukilani kuti panthawiyi , Davide anali atapha kale Uriya , munthu wosalakwa . ( Oweruza 4 : 24 ; 5 : 31 ) Cifukwa ca kukhulupilila Yehova Mulungu , Debora , Baraki , ndi Yaeli anadalitsidwa . Umu ndi mmene Baibulo lilili . Ngakhale zili conco , Akristu amene sangathe kupezeka pamisonkhano akhoza kucilikiza kulambila koona . Anthuwo angafune kufalitsa nkhani imeneyo panthawi ina , kapena mwa njila inayake . ( Luka 6 : 12 - 16 ; 22 : 2 - 6 , 31 , 32 ) Pamene ophunzila ake ena anamukhumudwitsa , Yesu sanaimbe mlandu Yehova kapena ophunzila ena osalakwa . ( Chivumbulutso 16 : 14 , 16 ) Komabe , zipembedzo zimaphunzitsa zinthu zosiyanasiyana , zosokoneza ndi zoopsa pa nkhaniyi . Tsunami ameneyu anacitika mu 2004 ndipo anapha anthu oposa 220,000 . 1 : 14 , 15 ) Zimenezi zimakhala zomvetsa cisoni kwambili cifukwa cakuti onse aŵili akanapewa kucimwila Yehova ngati akanamulola kuwathandiza kuona cikwati cao kukhala colemekezeka . Koma mmodzi wa iwo , “ Yudasi Isikariyoti , ” anam’peleka kwa adani ake . Mwacitsanzo , onani mbili ya moyo wa m’bale Trophim Nsomba mu Nsanja ya Mlonda ya April 15 , 2015 , masa . M’mipingo yambili , abale ayenela kulimbikitsidwa kuti ayenelele kukhala atumiki othandiza kapena akulu . Kuganizila zitsanzo zimenezi , kungatithandize kupindula na zinthu zimene zinalembedwa kale - kale kuti zitilangize . — Ŵelengani Aroma 15 : 4 . Pang’ono ndi pang’ono , n’naleka zaciwawa . Paulo anafotokoza kuti Hagara anali kuimila mtundu wa Aisiraeli , umene unacita pangano ndi Yehova kupyolela m’Cilamulo ca Mose . Ananipemphanso kuti niitane M’bale Frederick Franz kuti nayenso adzamvetsele zimene n’nali kuŵelenga . Nthawi zina , amayesa kulimbikitsa mamembala ao kuti azilalikila . Pa zaka zonse 27 zimene ndinali kupita kuchalichi , sindinamveko dzina la Mulungu ngakhale kamodzi . Mungaipeze mwa kucita skani QR khodi iyi kapena mungapite pa jw.org , ndi kulemba dzina la vidiyo imeneyi pa malo ofufuzila Lonjezo ili ndi ena ofanana nalo amatitsimikizila kuti anthu a Mulungu adzatetezedwa monga gulu . Mlongo ameneyu tsopano amalalikila uthenga wabwino ndi kuuzako ena ciyembekezo cabwino ca m’Baibulo . Mwacitsanzo , tinene kuti mwakhala ofooka osati cabe mlungu umodzi kapena iŵili , koma miyezi yambili . Pa cifukwa cimeneci , amuna Aciyuda sanali kukonda kulankhula ndi akazi . Colinga cake cinali cakuti [ Yosefe ] agone naye . ” Masiku ano , kagulu kocepa ka Ophunzila Baibulo kakula ndi kukhala Mboni za Yehova zokwanila 8 miliyoni . 22 : 20 ) Tikakangiwa kucita zimenezi , palibe cathu . Iye sanali kopotala ( mlaliki wa nthawi zonse ) , koma anali msilikali wacijelemani m’dziko la France . Ngakhale kuti cikondi “ cimakhulupilila zinthu zonse , ” ndipo sicikaikila ena , tiyenela kupewa kukhulupilila nkhani iliyonse yatsopano ndi yokondweletsa . ( Mlal . 7 : 20 ) Olo n’conco , tikalakwa sitiyenela kudziona monga olephelelatu kapena osatha kudzilanga tekha ngakhale pang’ono . Koma kodi zimenezi zinasonyeza kuti Mulungu walephela kulamulila anthu padziko lapansi ? Kodi tikambilana ciani m’nkhani ino ? Ni cenjezo lotani limene lilipo pankhani ya zosangulutsa ? Malinga ndi lemba la Salimo 15 : 3 , 5 , kodi Yehova amafuna kuti tizicita ciani kuti tikhale mabwenzi ake ? Mkristu wofikapo kuuzimu amatumikila bwino Yehova . Ganizilani zocitika zimene zingayambitse mikangano , ndipo pezani njila ya mmene mungazithetsele . Nayenso anali m’gulu la omasulila mabuku m’cinenelo ca Cifiji . Tsopano ndilinso ndi mzanga wokhulupilika , ndipo tikutumikila Yehova pamodzi mogwilizana . Timakondanso kwambili cinenelo . M’pempheni kuti akukhululukileni , ndipo yesetsani kubwezeletsa mtendele . “ Mawu a Yehova anamuyenga . ” ( Sal . Kukonda Mulungu , mkazi wanu ndi ana anu kudzakuthandizani kusamalila bwino banja lanu . ( a ) N’cifukwa ciani anthu a ku Galileya anafuna kumulonga ufumu Yesu ? Msampha wina wa Satana ndi ciwelewele . Anthu ena anali ndi maganizo olakwika ndiponso zolinga zolakwika . Munthu wovutika ine ! Limatilangiza ndi kutithandiza kuti tikhale oyenelela “ kucita nchito iliyonse yabwino . ” — 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 . Ali m’ndendemo , anakana kugwila nchito iliyonse yokhudzana ndi nkhondo . Anthu ambili amam’lemekeza Mulungu cifukwa cakuti analenga zinthu zakuthambo , za padziko lapansi , ndi anthu . Anzako ena asankha mapulojekiti ophunzila maulosi a m’Baibulo , kapena zimene Baibulo yakambapo pa nkhani zokhudza mbili yakale , zofukula m’matongwe , ndi za sayansi . Kodi tiyenela kupewa zosankha zotani ? Salimo 46 : 9 : “ [ Mulungu ] akuletsa nkhondo mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . Mwacitsanzo , ngati tiyang’ana pagalasi mofulumila , tingalephele kuona tolakwika twatung’ono koma tofunikila kukonza . Nkhani ya Kaini , Solomo , ndi ya Aisiraeli pa Phili la Sinai , zonse zili na mbali inayake yofanana . Eliya anafunika kulimba mtima kuti alankhule ndi munthu woipa ameneyu . Tangocita zimene tinayenela kucita . ’ ” Cofunika kwambili ndi mmene Mulungu amationela . Ena a io akugwila nchito m’cimango kapena analoŵa Sukulu ya Alengezi a Ufumu , ndipo ena akutumikila kumalo osoŵa . Mofananamo , kukula kwakuuzimu kumacitika mwapang’onopang’ono . Ndipo “ imfa yaciŵili ” imeneyi si mdani wa anthu amene amakonda Mlengi wao ndi kumtumikila . Miyambo 2 : 3 - 5 . Zosangulutsa zoipa ndiponso mabuku amene ali ndi zithunzi zoopsa , zimacititsa ana ndi acikulile kukhala ndi nkhawa . ( b ) Ndi vuto lotani limene Mkristu wina anakumana nalo ? Conco , Yefita sanali kutanthauza kuti adzapeleka munthu monga nsembe yeniyeni . N’kutheka kuti io anakhazikitsa makalasi amene anali kugwilitsila nchito kuphunzitsila anthu amenewo . Ngati ndinu wacinyamata ndipo mukufuna kucita zambili muutumiki wa Yehova , yesetsani kuŵelenga zofalitsa zathu zimene zili ndi nkhani zofotokoza mautumiki osiyanasiyana a nthawi zonse ndipo sankhani umodzi mwa mautumiki amenewa kuti ukhale colinga canu . Ngati timagwilizana ndi gulu la Yehova ndi kusamalila maudindo amene tapatsidwa , ndiye kuti ndife oyenelela kudzakhala mu Ufumu wa Mulungu . Tikuyembekezela moyo wosatha umene udzatipangitsa kukhala okhutila ndi osangalala . Tinali kutumikila monga woyang’anila dela wogwilizila ndi kucititsa misonkhano ikulu - ikulu . Kodi tingacite bwanji ngati taona kuti sitingathe kungonyalanyaza colakwaco ? Cilimbikitso cimene akulu amapeleka cingakuthandizeni kupilila . Conco , amafalitsa mabodza kuti acititse asilikali kuyamba kukayikila atsogoleli awo . Tikapeza munthu waukali mu ulaliki , tizikumbukila kuti mwina pali cam’khumudwitsa . 2 : 14 ) Nanga n’cifukwa ciani sanamvele Mulungu ? ( Mat . 5 : 37 ) Kumapeto a makambilano athu , tingam’funse nthawi yabwino imene tingabweleleko . Munthu wina wakale anati : “ Mulungu si munthu , woti anganene mabodza , si mwana wa munthu , woti angadzimve kuti ali ndi mlandu . Baibulo limayankha kuti : ndi kokha “ Mwa kudziyang’anila ndi kucita zinthu mogwilizana ndi mau [ a Mulungu ] . ” * Polamulila anthu ake , io anali kuimila Mulungu . Iye anauza asilikali a Isiraeli kuti asankhe munthu amene angamenyane naye , n’kumupha kuti nkhondo ithe . — 1 Samueli 17 : 4 - 10 . YEHOVA ndiye anayambitsa banja . ( Aef . Mwamuna wake anayamba kuphunzila Baibulo ndi kusonkhana na mkazi wake . Cisangalalo cake cakanthawi si cimwemwe ceni - ceni . — Miy . Pamene anali wacicepele , abale ake ansanje anam’gulitsa monga kapolo , ndipo om’gulawo anapita naye ku Iguputo . M’malo momuyankha mosaganizila bwino , coyamba tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi wacitila dala zimenezi ? N’cifukwa cake Yesu anacenjeza ophunzila ake kuti : “ Khalani maso ! 9 : 38 . Kodi Baibo ni yothandiza masiku ano kapena si yothandiza ? Anangonilola kupita , ndipo kucokela nthawiyo sananiitanenso . ” Zoona n’zakuti , Yehova “ sali kutali ndi aliyense ” amene amam’funafuna . Conco , n’zotheka kum’dziŵa . Popeza kuti nchito n’zosoŵa ndipo pali anthu ambili amene afuna nchito , anthu amene ali panchito amakakamizika kuseŵenza kwa maola ambili , mwinanso n’kumalandila malipilo ocepa . Nthawi zinanso , ena nyumba zawo zingawonongeke cifukwa ca tsoka la zacilengedwe , ndipo angafunikile malo okhala mpaka nyumba zawozo zitakonzedwanso . Ai , iye anasankha kucita zinthu zoyenela . Nchito zambili tsopano zimafuna kutsatila njila za sayansi yamakono zimene zimasintha mofulumila . Kodi timaona kuti amatithandiza pa umoyo wathu ? ( Agal . Mwina mungadzifunse kuti , ‘ Ngati Mulungu amadziŵa zonse , kuphatikizapo maganizo ndi zosoŵa zanga , n’cifukwa ciani ndiyenela kupemphela ? ’ ( b ) Nanga tidzakambilana ciani m’nkhani yotsatila ? ( Aroma 5 : 6 - 8 ) Dipo ndi umboni waukulu koposa wakuti Mulungu amatikonda kwambili . Ndipo n’cifukwa ninji ? ( b ) N’ciani cimene tifunika kucotselatu mumtima mwathu ? ( 1 Pet . Nicita ulaliki wa mumseu kuciyambi kwa zaka za m’ma 1950 MMENE BAIBULO LINASINTHILA UMOYO WANGA : Nthawi ina nditatuluka m’ndende , ndinaganiza zakuti ndikaone ang’ono a amai anga . 36 : 9 . 14 : 31 ) Iye n’citsanzo cabwino kwambili kwa ise pankhani imeneyi . Wophunzila Yakobo analemba kuti : “ Abale anga , sangalalani pamene mukukumana ndi mayeselo osiyanasiyana . ” ( Yak . 24 : 13 , 14 ) Conco , tiyeni tikambilane zifukwa zinayi za m’Malemba zimene timagwilila nchito yolalikila . Taonanso kuti ngakhale kuti Aisiraeli anali kulakwitsa zinthu zina , Yehova sanawasiye . Mboni za Yehova zinanionetsa cikondi ceni - ceni . Mbali ina inakhala India ndipo ina Pakistan . * Izi zinacititsa kuti anthu ambili ayambe kucita zaciwawa cifukwa cosiyana kwa zipembedzo . Kodi Baibo inapulumuka ku zinthu ziti ? 13 : 23 ) Timafuna kuona zinthu mmene Yehova amazionela na kumvetsetsa mfundo za m’Baibo . Zili conco cifukwa nthawi zambili ukalamba umabwela ndi zinthu zokhumudwitsa monga kusaoneka bwino , kufooka kwa thupi , vuto la kuiŵalaiŵala ndi matenda osatha . Iye anadadwa atadziŵa kuti n’covuta kwambili kulamulila mkwiyo wake . M’bale wina wa ku South Korea amasangalala akakumbukila nthawi imene anali kulandila abale na alongo oloŵa masukulu ophunzitsa Baibo . Kumapeto kwa moyo wake , Paulo analembela Timoteyo kuti : “ Ndikuyamika Khristu Yesu Ambuye wathu amene anandipatsa mphamvu poona kuti ndine wokhulupilika , ndipo anandipatsa utumiki . ” ( 1 Tim . 1 : 12 - 14 ) Ni utumiki uti umenewo ? Koma anthu ena amene timalalikila , saona conco . ( Yoswa 1 : 8 ) Cofunika kwambili ndi ‘ kugwilitsa nchito bwino nthawi yanu , ’ kutanthauza kucepetsako nthawi yocita zinthu zina zosafunika kuti muzisinkhasinkha Mau a Mulungu tsiku lililonse . — Aefeso 5 : 15 , 16 . Mkulu wa ansembe amene anaikidwa kukhala mfumu akuchedwa Mphukila . Cigwa ca Sidimu , cimene cinali m’dela la Dead Sea “ cinali ndi maenje ambili okhala ndi phula . ” — Genesis 14 : 10 . Patapita zaka 400 , Yehova anakamba mau awa ponena za iye mwini : ‘ Thanthwe , nchito yake ndi yangwilo , njila zake zonse ndi zolungama . ( Luka 10 : 25 - 27 ) Ndiye cifukwa cake , timatsatila citsanzo ca Kristu . Ifenso tinafikila kumeneko . Ndipo pambuyo pogulitsa katundu wina amene tinali naye , tonse anayi tinakwela honda ya Bob yakangolo kumbali pokasakila motoka yogula . Tinapeza motoka yakale koma yabwino . Tingaphunzile zambili pa nkhani ya Mfumu Solomo . Ambili aona kuti kukhala na umoyo wosalila zambili kumawathandiza kukhala acimwemwe , komanso kumawapatsa nthawi yokwanila yotumikila Yehova . KUONONGEDWA KWA DZIKO : Baibulo limakamba kuti Mulungu ‘ adzaononga amene akuononga dziko lapansi . ’ Tiyenelanso kuwathandiza kuganizila mfundo zimene tikuwaphunzitsa ndi kusankha okha zocita . Ndipo ayenela kuti anasangalala kwambili kuona kuti zopeleka zake zikucilikiza Yesu , ndi ophunzila ake 12 komanso ena amene anali kupita kukalalikila limodzi ndi Yesu . Kodi io amaiona bwanji nchito imene anasankha ? 101 : 3 ) Mwacitsanzo , M’bale wina asanakhale Mboni anali kukonda kupita kumaphwando kumene kunali kukhala mavinidwe oipa . 8 : 20 ; 18 : 19 ; Yobu 1 : 4 , 5 ) Komabe , Yehova kupyolela mwa Mose , anapatsa Aisiraeli malamulo amene anali kuwasiyanitsa ndi mitundu ina . N’cimodzi - modzi na Yehova . Iye amadziŵa kuti kum’patsa zina mwa zinthu zathu zamtengo wapatali kuli na ubwino wake kwa ise . Kucita izi kumalimbitsa kwambili ubwenzi wanu na iye . Malemba a Ezekieli 37 : 1 - 14 , ndi Chivumbulutso 11 : 7 - 12 , amanena za zinthu zimene zinacitika mu 1919 . Palibe mphatso yabwino imene makolo angapatse ana ao kuposa kuwathandiza kukhala pa ubwenzi wabwino komanso wolimba ndi Yehova . Ndi cuma cotani cimene tifunika kudziunjikila ? 2 : 1 - 5 , 12 , 13 , 18 , 19 ) Iye anauza mpingo wa ku Laodikaya kuti : “ Onse amene ndimawakonda , ndimawadzudzula ndi kuwalanga . Poyamba m’baleyo sanazindikile mphamvu ya moni wacidule umene anapeleka . Kuti anthu a nkhanza asinthe , afunika kuleka kukhala onyada , aumbombo , ndi odzikonda . ( Maliko 11 : 20 - 24 ) Nafenso tiyenela kutengela Yesu . Iye anabadwila m’dziko lina la ku Mexico , koma tsopano amasonkhana mumpingo wina ku Ulaya . Komabe , mfundo za m’Baibo zimaonetsa nzelu za Mulungu ndi cikondi cake pa ise . Vuto lina linali lakuti anali kusoŵa malo alendi okhala kwa nthawi yaitali . Koma cimakhala covuta kupilila ngati mavuto akupitilizabe ngakhale kuti timapemphela mocokela pansi pa mtima . Maboma a anthu alephelanso kubweletsa mtendele , citetezo , ndi cisangalalo ndipo aononga ngakhale dziko lapansi . Ngati nyumbayo ndi imene mukukhalamo , mukhoza kuipeleka komabe n’kupitiliza kukhalamo pa nthawi yonse imene muli ndi moyo . 11 : 28 - 30 ) Ndiyeno , anatsimikizila ophunzila ake kuti Mulungu anali kumvela cifundo wolambila Wake aliyense kuphatikizapo ‘ tiana ’ kutanthauza anthu amene dziko limaona kuti ndi osafunikila kwenikweni . — Mat . Ndithudi ! Yehova amatiteteza . ” Kuphunzila Baibo na mzimayi ameneyu kunalimbitsa kwambili cikhulupililo canga . Aliyense ayenela kuzindikila kuti ali ndi udindo , koma m’kupita kwa nthawi maudindo angasinthe , ndipo pangafunike kumasinthana zocita . Ngati zimenezo zikanakhala zoona , kodi sizingatanthauze kuti Mulungu ndiye acititsa zoipa zonse zimene zili paliponse m’dzikoli ? Njila yabwino ngako yodziŵila Mulungu na kukhala naye pa ubwenzi , ni mwa kuphunzila Mau ake , Baibo . Mwacitsanzo , apainiya anai ku Germany , anaganiza zolalikila m’gawo la malonda limene silinalalikidwe kwa zaka . Tili ndi zitsanzo zabwino za abale ndi alongo athu amene ali ndi cikhulupililo ‘ Mulungu Anakondwela Naye ’ ( Inoki ) , Na . Cinanso , mlongo wina mmishonale amene anatumikila ku Japan kwa zaka zoposa 30 , ananiitana kuti tikalalikile pamodzi m‘dzikolo kwa miyezi itatu . ( Yes . 49 : 15 ) Yehova amadziŵa mmene ena akumvela , ndipo nafenso watipatsa nzelu zotithandiza kuganizila mmene ena akumvela . — Sal . Nanga bwanji Mariya ? Mavuto amene anthu amakumana nao amasiyanasiyana , koma tingathe kuwalimbikitsa mwakuuzimu kapena kuwapatsa thandizo lina . — Ŵelengani Aroma 12 : 15 ; 1 Petulo 3 : 8 . Koma Baibulo silikamba kuti Paulo anamucilitsa . — Afilipi 2 : 25 - 27 , 30 . Zinthu zonsezi zimatipangitsa kukhala osiyana ndi nyama . 1954 mpaka 1956 , N’natumikila m’gulu la asilikali a United States kwa zaka ziŵili Lemba la 1 Akorinto 15 : 22 limati : “ Monga mwa Adamu onse akufa , momwemonso mwa Kristu onse adzapatsidwa moyo . ” M’nthawi yocepa cabe , anacilitsa munthu wopuwala dzanja ndi kubwezeletsa khutu la mwamuna wina limene linadulidwa . 35 : 8 . “ Zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inunso muwacitile zomwezo . ” — MAT . N’nayambadi kuphunzila , ndipo n’naloŵa m’gulu la nkhonya lochedwa Golden Gloves . Malemba anadzavumbulanso kuti Mulungu adzatumiza mmodzi wa m’gulu lakumwamba lili ngati mkazi wake , kuti “ akawononge ” Mdyelekezi . ( Mac . 6 : 1 - 6 ) Komabe , amuna amenewo ayenela kuti anali kale akulu asanapatsidwe udindo woonjezeleka umenewu . Mosakaikila Akristu anakumbukila mau a Yesu amene analembedwa ndi Luka . Yesu anati : “ Mukadzaona magulu ankhondo atazungulila Yerusalemu , mudzadziŵe kuti cionongeko cake cayandikila . ” Sanafune kungosanjikiza maudindo . 4 ) Apainiya ambili amalimbikitsiwa kwambili akadziŵa kuti ena mwa anthu amene iwo anawaphunzitsa coonadi akali kutumikila Yehova mokhulupilika , mwinanso kuti akucita upainiya . 15 : 22 . Mmishonaleyo anadabwa kwambili pamene banja lija linamuuza kuti anasiya kukoka fodya miyezi yambili m’buyomo . Mwina iye akudzifunsa kuti , ‘ Kodi ndidzacoka m’ndende muno ? N’cifukwa ciani muyenela kudalila Yehova kwambili ? Tikayesetsa kukhala okhulupilika , tidzakhala ndi mwai woona cocitika capadela kwambili kuposa zonse . Komanso Daniel , amene tamuchula kuciyambi , anati : “ Poŵelenga Baibo , nimasankha mavesi amene niona kuti adzakhala othandiza kwa anthu amene nimakumana nawo mu ulaliki . Kope ino ya magazini a Nsanja ya Mlonda , yoyamba pa makope apadela , idzakuthandizani kupeza mayankho pa mafunso amenewa . Imakamba za anthu eni - eni ndiponso malo eni - eni . ” Komabe , si anthu onse amene ali na makhalidwe oipa amenewa . 16 : 31 . Ndipo zimenezo zinalinso kukwanilitsa ulosi wa m’Baibo . ▪ Khalani ndi Banja Lolimba ndi Lacimwemwe Iye anati : “ N’nazindikila kuti moŵa sunali kuthetsa nkhawa zanga . Samueli atafika ku Giligala , anadzudzula Sauli . Mabwenzi amakondanso zinthu zofanana . Koma Yehova watipatsa ciyembekezo cosangalatsa . Kodi pempho la cakudya cathu calelo limaphatikizapo ciani ? ( Aroma 5 : 19 ; Aefeso 1 : 7 ) Cifukwa cakuti Mulungu analipila dipo limeneli , anthu ali na ciyembekezo codzasangalala na moyo wamuyaya m’paradaiso padziko lapansi . Omasulila mabuku odzipeleka amenewa amatsanzila abale a m’Bungwe Lolamulila , amene afuna kuti anthu azisamalidwa mwakuuzimu ngakhale kuti cinenelo cao cimakambidwa ndi anthu ocepa . Tingaonetse bwanji kuti ndife odzicepetsa ? ( Salimo 37 : 37 , 38 ) “ Munthu wosalakwa ” ndi amene amadziŵa Mulungu ndi Mwana wake ndipo amacita cifunilo ca Mulungu ndi mtima wonse ( Ŵelengani Yohane 17 : 3 . ) N’cifukwa ciani tingakhale na cikhulupililo cakuti Yesu adzatitonthoza ? Mamiliyoni a “ nkhosa zina ” za Yesu akuyembekezela mwacidwi mphoto ya mtsogolo ya moyo wamuyaya m’paradaiso padziko lapansi . Kodi mwamunayo anacita ciani pambuyo pake ? Joy anati : “ Iye wasintha ndipo amayesetsa kukhala mwamuna wacikondi potengela citsanzo ca Yesu . ” N’cifukwa ciani nkhanza ni yofala ? Koma mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika , dzina la Mulungu linabwezeletsedwa m’malo ake . Monga bambo uja amene anapempha Yesu kuti alimbitse cikhulupililo cake , nafenso tingakambe kuti : “ Limbitsani cikhulupillilo canga ! ” Kodi iye ndi mkazi wake akanaphunzitsa bwanji mwana wao kukonda Yehova ndi kum’tumikila popeza anthu ambili mu Isiraeli anali kucita zinthu zoipa pa nthawiyo ? Nikali kusangalala ndi maseŵela a baseball , koma siniwakonda kwambili ngati kale . Anthu ena ovutika . Davide analinso ndi anzake ena okhulupilika amene anakhala kumbali yake panthawi yovuta . Tifunika kuyesetsa kupeza nthawi yocita phunzilo laumwini ndi kupezeka pa misonkhano . Komanso , nthawi zina zinthu zokambidwa m’cinenelo ca makolo sizingamufike pamtima mwana . M’kupita kwanthawi , wophunzila wacidwi ameneyo adzamvela monga mmene wamasalimo anamvelela . Iye anaimba kuti : “ Kuyandikila kwa Mulungu ndi cinthu cabwino . Makolo ake ndiponso azilongosi ake atatu , onse anafa ndi cimpempho camphamvu cimeneco . Yesu anafotokoza fanizo la matalente poyankha zimene ophunzila ake anafunsa ponena za “ cizindikilo ca kukhalapo kwake ndi ca mapeto a nthawi ino . ” ( Mat . 1 , 2 . ( a ) Ni mtendele wanji umene tingakhale nawo palipano ? Ndi madalitso otani amene tidzapeza ngati tipanga zosankha zanzelu ? Nanga tifunika kucita ciani ? Mwacitsanzo , Mose anauza Aisiraeli kuti : “ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi mphamvu zako zonse . ” — Deut . ( 2 Akorinto 4 : 7 ) Mwacitsanzo , pamene Yesu anapempha kuti Atate ake acotse ciyeso cake , Yehova anatumiza mngelo kukam’limbikitsa kuti dzina la Mulungu lisacitidwe citonzo . Mlongo Wendy wa zaka za m’ma 60 , anayamba upainiya ali wacicepele ku Australia . Ndipo timakhulupilila kuti anaukitsidwa kwa akufa . Mwacitsanzo , buku lakuti Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo limafotokoza bwino kwambili za anthu 14 ochulidwa m’Baibulo . 13 : 44 ) Tikaona zotulukapo zabwino za kudzipeleka kwathu , cimwemwe cathu cimawonjezeleka , timakhala na umoyo wokhutila , ndiponso timathandiza ena kukulitsa cimwemwe cawo . — Mac . Tingacite ciani kuti tikhale acangu pa nchito imene tapatsidwa ? Iwo anamvetsela mabuku a Uthenga Wabwino akuŵelengedwa m’cinenelo cawo ca Cifulenchi , m’malo mwa Cilatini . Tate wabwino amasamalila ndi kuteteza ana ake . ( Mat . 13 : 10 - 15 ) Yesu anagwilitsilanso nchito mafanizo kuti anthu azikumbukila zimene anali kuwaphunzitsa ndi kuti azisangalala kumvetsela kwa iye . 7 : 1 . 26 Khalani na Cikhulupililo m’Malonjezo a Yehova 2 : 10 . 6 : 9 , 11 , 19 , 20 ) Tili ndi cidalilo cakuti Yehova adzatidalitsa monga mmene akutilonjezela . Ndiyeno , atumwiwo anali kugaŵila osowa ndalamazo . Ngakhale kuti n’nali na cibwenzi cimodzi cokha , n’nalinso kuyenda ndi akazi ena , komanso n’nali cakolwa . Mu 1950 tinakwatilana , ndipo podzafika mu 1953 tinali ndi ana aŵili . Iye anatipulumutsadi ku cinthu coopsa , ndico imfa . ” — 2 Akor . Komabe , malemba opanda macaputala ndi mavesi amenewa anali ndi vuto lake . Pamene n’nali mwana , amayi ananiphunzitsa kupemphela usiku uliwonse . “ MTIMA WANGA WAGALAMUKA CIFUKWA CA NKHANI YOSANGALATSA ” 3 , 4 . ( a ) Kodi ndi “ nkhani yosangalatsa ” iti imene imatikhudza ? ‘ Kodi wanilakwila kwambili cakuti afunika kunipepesa , kapena niiŵaleko cabe ? ’ Angatiuzenso kuti tizidya kapena kupewa kudya zakudya zina . Kodi ndinu wacinyamata ndipo mukufuna kubatizidwa ? Pa January 1 , 1956 , n’nayamba kutumikila monga mpainiya wanthawi zonse . Zimene mumacita bwino : Kodi nili na maluso ati ? Koma wa Mboni za Yehova anandiyankha mafunsowo pogwilitsila nchito Baibulo . Iye anakamba motsimikiza kuti Mulungu ‘ sangacite zimenezo ayi . ’ Kodi Aramagedo n’ciani ? Pambuyo pake , Satana “ anagwetsela Yobu zilonda zopweteka , kuyambila kuphazi mpaka kumutu . ” — Yobu 1 : 7 - 19 ; 2 : 7 . ▪ “ Mudzakhala Mboni Zanga ” Kukhala woceleza ni mankhwala amphamvu othetsela vuto la kusungulumwa . Kodi mungathandize bwanji ena ndi cidziŵitso cimene mwapeza cifukwa cotumikila kwa zaka zambili ? Kukambilana ndi acicepele kumakhala kovuta , maka - maka azaka pakati pa 13 ndi 19 . Koma Carol anali wovuta ndipo sanali kuyamikila ngakhale kuti Lily anali kumucitila zinthu zambili zabwino . Panthawi imene buku la Yeremiya linali kulembedwa , ufumu wakumpoto wa mafuko 10 unali utagonja kale kwa Asuri , ndipo anthu ambili a mu ufumuwo anali atatengedwela ku ukapolo . Yehova afuna kuti oipa acenjezedwe ponena za zotsatilapo za njila zao zoipa . — Ezek . Kodi Mose na Aroni anaonetsa bwanji kuti anali ku mbali ya Yehova ? ( Mac . 27 : 24 ) Kuciyambi kwa ulamulilo wake , Nero , Mfumu ya Roma , anakambilatu kuti sadzaweluza milandu yonse payekha . Kuti atelo amafunika kuganizila kalembedwe ka Ciheberi , mavesi apambuyo ndi patsogolo , na malemba ena ogwilizana ndi nkhaniyo . Ngakhale kuti munthu wa conco anganamize anthu kwa kanthawi , Yehova Mulungu wamkulu ndi wacilungamo amatiuza kuti , “ wobisa macimo ake zinthu sizidzamuyendela bwino . ” — Miy . 28 : 13 ; ŵelengani 1 Timoteyo 5 : 24 ; Aheberi 4 : 13 . Ndipo zimenezi zizionekela kwa anthu ena . Kudzipeleka kuti tithandize ena , nthawi zina kumakhala kovuta . Luso lomvetsa ndi kukamba cinenelo ndi mphatso imene Yehova anatipatsa . Mtumwi Paulo , amenenso analipo pa msonkhano umene unacitika ku Yerusalemu mu 49 C.E . , anakumana ndi Petulo ku Antiokeya , ndipo anam’dzudzula cifukwa ca zaciphamaso zimene anacita . ( Mac . 15 : 12 ; Agal . Nthawi zina anthu ambili a kumaloko samapezeka pa nyumba . Ganizilani citsanzo ca Paulo . Lemba la Luka 2 : 37 limakamba kuti : “ Sanali kusoŵa pakacisi . Anali kucita utumiki wopatulika usana ndi usiku , anali kusala kudya ndi kupeleka mapembedzelo . ” Atafufuza m’mabuku ofotokoza mbili yakale a m’nyumba yacifumu , anapeza umboni wakuti zimene Ayuda anakamba zinali zoona . Mwacitsanzo , bwanji ngati munthuyo akamba kuti samakhulupilila Mulungu ? Koma pambuyo pa zaka zocepa , mpingowo unakula mofulumila ndiponso modabwitsa kwambili . Ngati iye amawakonda , nanga ise n’kulekelanji kuwakonda ? Bungwe la World Food Programme inati : “ Dzikoli lili na cakudya cokwanila kudyetsa munthu aliyense , koma pa anthu 815 miliyoni , mmodzi pa anthu 9 alionse amagona na njala tsiku lililonse . Ndinakhala ndi cikumbumtima cabwino cifukwa coŵelenga Malemba monga Miyambo 11 : 1 limene limakamba kuti ‘ masikelo acinyengo amam’nyansa Yehova . ’ ” N’ndani wa ise amene sanakhudzidwepo na nkhondo , umphawi , kapena kusankhana mitundu ? 5 : 16 - 26 ; Aef . Ayenela kuti anali ataganizapo kutelo . ( b ) Nanga n’cifukwa ciani iye anamva conco ? ( b ) pa nchito za masiku onse ? Nchito yolalikila ndi kuphunzitsa yapadziko lonse imeneyi , yathandizanso anthu ambili kudziŵa kuti Mboni za Yehova ndi otsatila oona a Kristu Yesu . Koma kodi io amaona kuti sanasankhe bwino kukatumikila pa Beteli ? D , limafotokoza bwino maonekedwe a Paulo , mogwilizana n’zimene anthu anali kukhulupilila kwa nthawi yaitali . Pamene Elifazi wa ku Temani anafunsa Yobu mafunso amenewa , mwacionekele anali kukhulupilila kuti yankho lake n’lakuti ayi . Merozi anatembeleledwadi , ndipo masiku ano n’zovuta kudziŵa kuti Merozi anali ciani . Cifukwa cakuti mukamaonetsa kuti ndinu okhulupilika ndiponso odalilika , akulu adzadziŵa kuti Yehova afuna kukupatsani maudindo ena oonjezeleka mumpingo . — Sal . 101 : 6 ; ŵelengani 2 Timoteyo . 2 : 2 . ( a ) Ni mafunso ati amene tifunika kudzifunsa ? Kodi sitikuyembekezela mwacidwi nthawi yosangalatsa imeneyo ? — Ŵelengani 2 Petulo 3 : 13 . Kukamba zoona , alongo osakwatiwa amene akutumikila kumaiko acilendo akhala na mbili yabwino ngako mu utumiki wawo wacikhiristu . Okalamba okhulupilika amenewa angakhale ndi cidalilo cakuti Mulungu adzayankha mapemphelo ao . Kodi mungasonyeze bwanji kudekha pa zocitika izi ? Tiyelekezele kuti muli ku nchito , ndiyeno woyang’anila sakugwila bwino nchito yake . Iye anabweletsa mabuku amene ndinapempha ndi kundipempha kuti tiziphunzila Baibulo , ndipo ndinavomela . Kodi Kristu adzapambana pa nkhondo yolimbana ndi adani ake motsatila ndondomeko yotani ? M’malo mwake , io ‘ amapitiliza kukhala ndi akazi ao mowadziŵa bwino , ndi kuwapatsa ulemu monga ciwiya cosalimba . ’ ( 1 Pet . M’kupita kwa nthawi , Johannes Gutenberg atayamba zopulinta - pulinta , akatswili ambili a Baibo anayamba kutulutsa ma Baibo osiyana - siyana m’zinenelo zambili zimene anthu anali kukamba zungulile Europe yonse . Iye anafunika kugonjetsa asilikali amphamvu a mitundu yokhala m’dzikolo . 13 : 2 ) Lomba tiyeni tikambilane mafunso otsatilawa : Kodi Yehova amawaona bwanji alendo ? Timakonda kuuka mwamsanga , ndipo cizoloŵezi cimeneci cimathandiza pa Beteli . 40 : 26 ) Ndipo sikuti Yehova ndi Yesu amangokumbukila amene anamwalila koma amafunitsitsa kudzawaukitsa . Kodi tiyembekezela zotani m’tsogolo ? Koma ndimakwanitsa kuŵelenga Baibulo tsiku lililonse , kupita kumisonkhano , ndi mu ulaliki . Kodi mwayesapo kale ena a io ? Pitilizanibe kutumikila Mulungu mwacimwemwe . Zinthu zimene zingatilepheletse kupita patsogolo mwauzimu . ( Aroma 5 : 19 ) “ Munthu mmodziyu , ” ndi Yesu . Ambili a ise tinacitilidwapo nkhanza ndi anthu oipa monga aciwawa , odana ndi anzawo , ndi zigaŵenga zoopsa . 11 / 15 Atandifunsa ngati ndikufuna kudziŵa zambili , ndinavomela mokondwela . ” — Koffi , Benin . NKHANI YA PACIKUTO | MUNTHU AMENE MUMAKONDA AKAMWALILA Ndipo amuna 6 onyamula zida zophwanyila anauzidwa kuti aphe anthu onse a mumzinda amene sanaikidwe cizindikilo . M’kuluyo anagwila mau a pa 1 Timoteyo 3 : 1 ndi kumuuza kuti , akulu alandila kalata yoonetsa kuti iye wayamikilidwa kukhala mkulu . ( Luka 22 : 28 - 30 ) Pangano limeneli linawatsimikizila kuti adzalamulila naye limodzi kumwamba . — 10 / 15 , tsamba 16 - 17 . Kodi si ine , Yehova ? ” — Eks . Nthawi zina , tingafunikile kupeleka ndalama zothandizila pa nchito yokonzanso ofesi yathu ya nthambi , zocilikizila msonkhano wacigawo , kapena zothandizila abale athu amene akhudzidwa na tsoka la zacilengedwe . Anali kum’phikila , kum’capila , ndi kusamalila acibale ena a mwamuna wakeyo . Kodi anthu ambili akamba ciani pambuyo polandila Baibulo la Dziko Latsopano lacingelezi lokonzedwanso ? Njila yaikulu imene timaonetsela kuti timayamikila dipo , ni mwa kudzipeleka kwa Yehova cifukwa cokhulupilila dipo na kubatizika . Mneneli Danieli analemba kuti m’nthawi ya mapeto , “ anthu ozindikila , ” kapena kuti odzozedwa , ‘ adzathandiza anthu ambili kukhala olungama . ’ Kuti tikhale na cikhulupililo cokwanila , tifunika cidalilo cakuti Mulungu amapeleka mphoto kwa amene amam’funa - funa mwakhama . N’cifukwa cake Baibo imati “ cikhulupililo ndico ciyembekezo cotsimikizika ca zinthu zoyembekezeledwa . ” ( Aheb . Nthawi ina , io anandiuza kuti ndiwafotokozele kumene kuli likulu lathu . Nanga Abulahamu anacita ciani ? Ngakhale kuti anthu ambili a ku Japan salidziŵa bwino Baibulo , io ali ndi cidwi cofuna kuliŵelenga . Antonio anapeza thandizo lofunikila , ndipo tsopano analeka khalidwe lake loipalo . ( Genesis 2 : 19 , 20 ) Kuyambila panthawiyo , anthu a Mulungu akhala akutamanda Yehova ndi kuuza ena za iye mwakugwilitsila nchito cinenelo . 3 : 10 ) Cifukwa cakuti Timoteyo anali kuseŵenzetsa zimene anaphunzila kwa ena , anakhala woyenelela kulandila udindo wina waukulu . — 1 Akor . Kuyamikila dipo kuyenela kutisonkhezela kucita zonse zimene tingathe kuti tithandize ena kudziŵa kuti nawonso angapindule ndi mphatso ya mtengo wapatali imeneyi . Iye akuwauza kuti Yehova anadalitsa kwambili Abulahamu ku Kanani , ndi kuti Abulahamu ndi Sara ali ndi mwana dzina lake Isaki amene anali kudzalandila coloŵa ca atate ake . Komanso , munthu wobwezela magazi sanali kuloledwa kuloŵa mumzinda wothaŵilako kuti akaphe wothaŵayo . ( 1 Akorinto 5 : 11 ; 2 Yohane 9 - 11 ) Ndiyeno , m’kalatayo , iye mokoma mtima anawafotokozela kuti io ndi amene anakhumudwitsa banja lao cifukwa cakuti anacimwa ndipo sanalape . Kodi uphungu wa m’Mau a Mulungu umatithandiza bwanji kukhala aukhondo , amtendele , ndi ogwilizana ? Mzimu Woyela wa Mulungu . Akhiristu a ku Roma anafunika kutengela citsanzo cake . Atate anamwalila kutatsala miyezi 6 kuti nibadwe , ndipo Amayi anamwalila nikali khanda . Ngati iye sakumwetulila , ndiye kuti mwina pali cinacake cimene cikumuvutitsa maganizo , ndipo kungomumvetsela pamene akamba nkhawa zake kungamulimbikitse . — Yak . Lembali limapezeka kangapo konse m’buku yakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse . 22 : 39 ) Cikondi cimeneci cimatilimbikitsa kupitiliza kugwila nchitoyi , podziŵa kuti anthu ena angayambe kumvetsela uthenga wathu pamene zinthu zasintha mu umoyo wawo . ( Sal . 73 : 24 ) Ngati tifuna kuti Yehova atitsogolele , ‘ tizim’kumbukila ’ mwa kufufuza m’Baibulo kuti tidziŵe malingalilo ake . Tingacite ciani kuti ‘ timvetsetse ciliconse ’ cofunikila kuti tikondweletse Atate wathu wakumwamba ? Yehova anamuuza kuti apite kwa Farao kuti akapulumutse anthu a Mulungu opondelezedwa , amene anali akapolo ku Iguputo . Pambuyo pakuti atumwi onse amwalila , mpatuko umenewo unafalikila , ndipo unayambitsa Machalichi Acikristu . Motelo , n’zosadabwitsa kuti ngati anthuwo akana mphatsoyo , ‘ mtima umatipweteka . ’ MOUZILIDWA , mtumwi Petulo anagwila mau a m’buku la Levitiko . Iye anafotokoza kuti Akristu ayenela kukhala oyela monga mmene Aisiraeli anafunikila kukhalila oyela . Pokamba ndi Atate ake , Yesu anati : “ Atate ndikukutamandani pamaso pa onse , inu Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi , cifukwa zinthu izi mwazibisa kwa anzelu ndi ozama m’maphunzilo , koma mwaziulula kwa tiana . ” Kodi hachi yoyela imene Kristu wakwelapo imaimila ciani ? Ndiponso zapangitsa kuti zofalitsa zathu zizitulutsidwa m’zinenelo zambili kuposa kale . “ Nditamva mabelu ocenjeza , ndinapita kukabisala ndipo ndinagona pansi apo n’kuti mabomba akuphulika . Ici cingakhale ciyeso cacikulu . Panthawi imeneyo n’napeleka pemphelo lacidule kwa Yehova , n’kumupempha kuti anithandize kupilila . Baibulo lathandiza anthu ambili kusintha umoyo wao . Monga mmene cisote cimatetezela mutu na ubongo wa msilikali , “ ciyembekezo cacipulumutso ” cimateteza maganizo athu , na kutithandiza kuti tiziganiza bwino . ( 1 Ates . Pamene m’bale akamba nkhani mumaganizila mlendo wanuyo . 2 : 7 ) Iwo ndi amtengo wapatali cifukwa ca kukhulupilika ndi kudzipeleka kwao . ( Agalatiya 6 : 1 ) M’malomwake , iwo amapempha Yehova kuti awapatse nzelu ndi luso lomvetsa zinthu . Cimaniŵaŵa kuona kuti mphamvu zanga ziyenda zisila . N’ciani cidzacitikila Satana ? Iye anati : “ Kumbali yake , Mariya wasankha cinthu cabwino kwambili , ndipo sadzalandidwa cinthu cimeneci . ” Iwo akana mau a Yehova . Kodi ali ndi nzelu yotani tsopano ? ” Jean - David ( pakati ) Komanso kupilila kumathandiza munthu kuona mavuto moyenela ndi kuika maganizo pa colinga cake , osati pa kupweteka kwa mavutowo . Kukhala okhulupilika kwa Yehova kumafuna kucita zinthu molimba mtima anthu akatiopseza . Koma nthawi iliyonse imene anthu ena anali kupita kukamucezela , iye anali kulankhula nao za m’Malemba ndi kuwalimbikitsa mwakuuzimu . — Mac . Lembani zinthu zitatu zimene mufuna kuti mnzanu wa m’cikwati azicita , zoonetsa kuti amakulemekezani . ( Aroma 13 : 7 ) Koma ngati boma latilamula kucita zinthu zimene Mulungu amaletsa , timakana mwaulemu . N’cifukwa ciani m’busa anakamba kuti wokondedwa wake anali “ ngati munda wochingidwa ndi mpanda ” ? Kodi munaganizapo zakuti muŵelenge Baibo , koma munagwa mphwayi cifukwa cokhala na maganizo olingana ndi a anthu amene tawachula pamwambapa ? Komabe , nchito yake inathandiza kwambili . Iye sanafune kukhala wodziŵika m’dzikoli , koma anafuna kukhala wodziŵika kwa Atate wake . ( Aheb . Conco , ngakhale kuti munthuyo anali wamoyo , anali ngati mtembo cifukwa anaweluzidwa kuti anyongedwe . M’bale Sergio na mlongo Olinda , amene tawachula poyamba paja , anadzionela okha kusintha kwa conco . Yesu sanadodome kufunsa otsatila ake zimene anali kukhulupilila . ( Mat . Kuti tipitilize kuyenda m’coonadi , tiyenela kumvetsela zimene Yehova amatiuza . Mzindawu unali m’dela limene Aperisiya anali kulicha kuti Tsidya Lina la Mtsinje , kutanthauza kumadzulo kwa Firate . Ngakhale n’telo , ndine wosangalala tsopano . Genesis caputa 11 - 24 ; onaninso 25 : 1 - 11 ( Sal . 15 : 4 ) Ngati tavomela kukaceza ku nyumba kwa wina wake , sitifunika kusintha maganizo popanda zifukwa zomveka . NYIMBO : 89 , 26 Machitidwe 20 : 1 , 2 imati : ‘ Cipolowe . . . citatha , Paulo anaitanitsa ophunzila . Atawalimbikitsa na kulailana nawo , ananyamuka ulendo wopita ku Makedoniya . N’cifukwa ciani mtumwi ameneyu anali wotsimikiza kuti Yesu ali moyo ? Mariya Mmagadala atamuona , anaganiza kuti anali wosamalila munda ; ndipo ophunzila ake aŵili amene anali kuyenda ku Emau , anaganiza kuti ni mlendo . — Luka 24 : 13 - 18 ; Yohane 20 : 1,14 , 15 . Ngakhale kuti nthawi zina Petulo anaoneka kuti anali ndi maganizo osakhazikika , Yesu anam’lonjeza kuti iye adzakhala wokhazikika monga thanthwe . — Yoh . Zimenezi zikakucitikilani , muzikumbukila citsanzo ca munthu wa m’fanizo la Yakobo . 8,050,000 Paulo anapeleka moni kwa Akhristu anzake ambili . Kupatula anthu odwala matenda oyambukila . Monga mmene Petulo anacitila , nafenso tiyenela ‘ kuyang’anitsitsa ’ Yesu . Koma kodi tiyenela kucita ciani ngati talephela kukhazikitsa mtendele ? Koma zikadzadziŵika kuti ucifumu wa Yehova ndiwo wabwino , onse adzagonjela ulamulilo wake wolungama kwamuyaya . Lije , amene lomba ni woyang’anila dela , anati : “ Anthu ambili kumeneko anali malova . Anthu masauzande anakhudzidwa kwambili ndi uthenga umene Yesu anali kulalikila ndiponso khalidwe lake . ( Luka 13 : 1 - 5 ) Kodi n’canzelu kuganiza kuti Mulungu amakonzelatu amene adzapulumuka ndi amene adzafa pa zinthu zotigwela mwadzidzidzi ? Odzozedwa a m’gulu laciŵili la “ m’badwo uwu ” anadzozedwa ndi mzimu woyela panthawi imene odzozedwa a m’gulu loyamba anali ndi moyo padziko lapansi . Koma kukumbukila mmene timaonekela pa maso pa Mulungu ndi kutsatila mapazi a Mwana wake kungatithandize kukhala odzicepetsa . Ngakhale ndi conco , Yehova ndi woleza mtima . Olaudah Equiano , kapolo amene anapulumuka , anati : “ Zimene tinakunana nazo zinali zomvetsa cisoni kwambili cakuti zinali zovuta kuzifotokoza . ” Kutengela makhalidwe a Yehova kumatenga nthawi . Mwacitsanzo , pokamba za JW Broadcasting , m’bale wina na mkazi wake , amene akutumikila m’dziko lina ku Asia , analemba kuti : “ Timatumikila m’tauni inayake yaing’ono . Kodi ofalitsa amagaŵila bwanji bukuli ? Mwacibadwa , kodi anthufe timafuna ciani ? Ngakhale nditakula , zinali kundivuta kuwasonyeza mmene ndinali kumvelela . Ndinali kuba macola , m’nyumba zamdadada ndi kuthyola nyumba zikuluzikulu usiku . N’zosacita kufunsa kuti Davide anapemphela mocondelela pamene anali kutola miyala 5 yosalala ing’ono - ing’ono m’mbali mwa mtsinje wouma wa m’cigwaco . Mkazi wa Potifara anayamba kukhumbila Yosefe , amene anali “ wokongola m’maonekedwe ndi wa thupi loumbika bwino , ” mwakuti anamunyengelela mobweleza - bweleza kuti agone naye . ( Ŵelengani Yeremiya 31 : 31 - 34 . ) Patangopita zaka zocepa , amayi anayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . Nikaganizila zakale , nimakumbukila zimene n’nali kuphunzila m’Baibulo . Baibo imati : “ Akalonga a Isiraeliwo ndi mfumuyo atamva zimenezi , anadzicepetsa n’kunena kuti : ‘ Yehova ndi wolungama . ’ ” Aheberi anali kuona kuti tsiku limayamba dzuŵa likaloŵa ndi kutha tsiku lotsatila dzuŵa likaloŵa . Kodi ofalitsa anafunika kuphunzitsidwa ciani ? Nanga ndi sukulu iti imene yawathandiza kukhala alaliki ogwila mtima ? N’cifukwa ciani tiyenela kuphunzila makhalidwe a Mulungu ndi njila zake ? Mwana woyamba wa Rakele anali Yosefe . Tsopano , Erica ndi wokondwa kutumikila monga mpainiya wapadela ku Ebeye pazilumba za Marshall . Pasanapite nthawi yaitali , apolisi anayamba kubwela kunyumba kwathu kudzafuna - funa mabuku ophunzilila Baibo . Koma , Baraki anayembekezela citsogozo kucokela kwa Yehova kudzela mwa Debora . NYIMBO : 54 , 36 ( Numeri 30 : 2 ) Monga munthu wokhulupilika Hana , amene ayenela kuti analiko panthawiyo , Yefita anasunga lonjezo lake , ngakhale anadziŵa kuti zidzakhala zovuta kwa iye ndi mwana wake . Visote vina vinali kukhala na cogwilila kotelo kuti nthawi zina msilikali anali kucinyamula kumanja . Yehova anauza Habakuku kuti ayenela ‘ kuyembekezelabe . ’ — Ŵelengani Habakuku 1 : 1 - 4 ; 2 : 3 . ( Yes . 46 : 10 , 11 ; 55 : 11 ) Conco , ndife otsimikiza kuti colinga ca Yehova ca poyamba cidzakwanilitsika ndendende panthawi yake . Mwina mumapemphela kwa Mulungu kuti akupatseni mphamvu ndi nzelu . “ Pali nthawi ‘ yovomeleza kuti cinthu catayika . ’ . . . Kumbukilani kuti Mulungu analimbitsa Asa ndi kum’thandiza , ndipo inunso adzakulimbitsani . Kenako anati : “ Ndani ali kumbali ya Yehova ? Kodi atumiki a Yehova athandiza bwanji pa nchito yomasulila Baibulo ? Luso limenelo ‘ lidzakuyang’anila ’ na kukucinjiliza ku ziphunzitso zimene zingawononge cikhulupililo cako . — Ŵelengani Miyambo 2 : 10 - 12 . Ndiyeno , Mboni ya Yehova inasonyeza Yeong Sug mau a m’Baibulo awa : “ Pakuti amoyo amadziŵa kuti adzafa , koma akufa sadziŵa ciliconse . Ganizilani za mlongo wina amene mwana wake wamkazi anacotsedwa na kucoka pa nyumba . kuona mmene Yehova amalimbikitsila anthu ake kupitila m’Mau ake ? Mwina mumpingo mwanu muli m’bale amene kakambidwe kake na zocita zake zimakukhumudwitsani . Mwacitsanzo , nthawi zina mwininyumba sanali kugwilizana ndi uthenga umene wamvetsela pa galamafoni . Mapeto ali pafupi kwambili . Conco , apa ndiye pamene tiyenela kulalikila kwambili uthenga wabwino . [ Bokosi papeji 26 ] Anapeleka Thandizo Loyenela Ndiponso , taonako mbali yocepa cabe ya cilengedwe cake . ( Mlal . Ŵelengani Yesaya 40 : 31 . Zitsanzo zimenezi zionetsa kuti atumiki ena a Yehova anacitapo zolakwa zimene zinakhumudwitsa kwambili anthu ena . Kodi Yehova amafuna kuti anthu amene maina awo analembedwa ‘ m’buku lacikumbutso ’ azicita ciani ? Dziko lapansi linapangidwa kuti likhale malo abwino okhalamo anthu amene amalemekezana ndi kukonda Mlengi wao . Kodi ciyembekezo ca ciukililo cili ndi tanthauzo lotani kwa inu ? Mau a Mulungu amati : “ Kwa munthu , palibe cabwino kuposa kuti adye , amwe , ndi kusangalatsa mtima wake cifukwa coti wagwila nchito mwakhama . ” ( Mlal . Iye anali kudziŵa kuti Timoteyo anali ndi manyazi ofunika kuwathetsa . Kudziŵa mmene Yehova amakhalila mfumu n’kofunika kwambili . 3 : 13 , 14 ) Komanso “ cikondi n’coleza mtima ndiponso . . . sicisunga zifukwa . ” ( 1 Akor . Tonsefe timasangalala kupezeka pa misonkhano yampingo , yadela , ndi yacigawo . Ndipo iye ndi mmodzi mwa anthu osangalala kwambili . ” Pa cifukwa cimeneci , mu September 2007 , Bungwe Lolamulila linapeleka cilolezo cakuti Baibulo la Dziko Latsopano la Cingelezi likonzedwenso . Kodi tauona umboni woonetsa kuti wokwela pa hosi yakuda ali pa liŵilo kucokela mu 1914 ? Ndipo mwina anadzifunsa kaya ngati Yehova anali kusiyanitsa Akristu okhulupilika ndi Akristu acinyengo . — Mac . 20 : 29 , 30 . 11 : 24 - 26 . Mu June 1966 , kunali mlandu wapadela m’khoti ya ku Lisbon . NKHANZA ZA PANYUMBA NDI KUGONEDWA MWACIKAKAMIZO : “ Mkazi mmodzi pa akazi atatu aliwonse , anacitidwapo nkhanza ya panyumba kapena kugwililidwa ndi mnzake wa pamtima nthawi ina pa umoyo wake . ” Inatelo lipoti ya United Nations . Koma kodi na abale a pa udindo cabe amene ayenela kulimbikitsa ena , monga mmene Yehova amacitila ? ( a ) Tingawathandize bwanji abale athu kupita patsogolo ? Akulu ena atumikila mumpingo modzipeleka kwa zaka zambili . Koma anapeza citonthozo cacikulu pa mau apa Salimo 94 : 19 . Pa lembali wamasalimo anauza Mulungu kuti : “ Malingalilo osautsa atandiculukila mumtima mwanga , mau anu otonthoza anayamba kusangalatsa moyo wanga . ” ( b ) N’cifukwa ciani nthawi zina kusinkhasinkha n’kovuta ? Cifukwa cakuti anali kufuna kuthandiza “ anthu onse , ” Ayuda ndi anthu ena , kuphunzila coonadi kuti akapulumuke . ( Aroma 3 : 10 ; 9 : 29 ) Zinali zovuta kudziŵa pamene mauwo akupezeka ngati simukudziŵa bwino “ malemba oyela . ” ( Mateyu 24 : 14 ; 28 : 19 , 20 ) Tiyenela kuitana anthu onse a “ ludzu ” kuti adzamwe “ madzi a moyo , ” kutanthauza kuti tiyenela kuphunzitsa anthu amene afuna kumva coonadi ca m’Baibulo . Koma , “ Nowa anali munthu wolungama . Pafupifupi mwezi wonse , iye anali kukhala pansi kuŵelenga mobwelezabweleza kufikila ataloŵeza nkhani yonse pamtima . Iye atachula za “ kusamvela makolo , ” anachula za kusayamika . Anthu osayamika amasuliza zabwino zimene ena amawacitila . Popeza kuti anali kufuna kucita zambili potumikila Yehova , analeka nchitoyo ndi kuyamba upainiya . ( Mateyu 24 : 13 ) N’ciani cimene cingathandize acinyamata kukonzekela kuti atumikile Yehova kwamuyaya ? “ Koma Mau a Mulungu ndi mzimu wake woyela zinatithandiza kusankha zocita mwanzelu . Ndi udindo wathu kuuza anthu za uthenga wabwino . — Mac . Akulu , Kodi Mumakonda Kuphunzitsa Ena ? ( 1 Akor . 10 : 25 , 29 , 30 ) Cotelo , pa nkhani yaikulu imeneyi yokhudza kulambila , Mkhiristu aliyense anafunika kupanga cosankha mogwilizana ndi cikumbumtima cake . Panthawi ina yake , anali kuphunzila ndi anthuwo m’magulu cifukwa manyumba awo anali oyandikana . Cikondi ca a·gaʹpe cimaphatikizapo kukhala wokoma mtima ndi waubwenzi . Koma cimaonekela kwambili mwa zocita zathu zoonetsa kuti timaganizila anthu ena . Ngati ana ndi akulu amakambilana bwino - bwino zingathandize kusamalila makolo okalamba . ( b ) Kodi inuyo mwapindula bwanji ndi maphunzilo amene mwalandila ? 1 : 31 ; Yer . 10 : 12 ) Tingaphunzilepo ciani tikaona mmene cilengedwe cilili cokongola ndi cadongosolo ? Komabe , posacedwapa anthu omvela adzakhala m’dziko labwino lopanda ziphuphu kapena umphawi . Caka catha , anthu 19,862,783 anapezeka pa cocitika cimeneci . Kuyamikila abale athu mocokela pansi pamtima kungakhale ndi zotsatilapo zabwino . Masiku ano , ambili ali ngati Davide . ( b ) Nanga ni madalitso anji amene tiyembekezela ? Tsiku ndi tsiku timafunika kukhululukidwa macimo , ndipo ndife okondwa kuti Yehova anatipatsa nsembe ya dipo la Yesu imene imatheketsa kuti macimo athu akhululukidwe . David Sinclair Mwa thandizo la Yehova , ngakhale ise anthu opanda ungwilo tikhoza kum’gonjetsa Satana . ( 1 Yoh . Kodi mungagwilitsile nchito nkhaniyi kudziyesa kuti muone ngati mukali m’cikhulupililo ? Nkhani ya pa Ekisodo imati : “ Yehova anamufunsa [ Mose ] kuti : ‘ Cili m’dzanja lakoco n’ciani ? ’ Ndipo si zokhazo ai , iye anatilenganso m’njila yakuti tizitha kusangalala ndi zakudya . ( Mlal . ( Ezek . 38 : 11 ) Apa m’pamene mau a Yesu adzakwanilitsidwa , akuti : “ Pa nthawi imeneyo olungama adzawala kwambili ngati dzuŵa mu ufumu wa Atate wao . ” — Mat . 26 : 3 - 5 ; 35 : 11 ) Koma izi zisanacitike , mbadwa za Yakobo zinakhala akapolo ku Iguputo . Koma si acinyamata onse a m’nthawi za m’Baibulo amene anali osayamikila . Taganizilani cisangalalo cimene anali naco pamene anali kuyenda - yenda m’mundamo poganizila kuti adzakhala ndi munda wabwino . N’cimodzi - modzi na ise . Zipatso zimene timabala si ophunzila atsopano , koma ni mbewu zatsopano za Ufumu . Tikacita zimenezo , tidzapewa kuononga nthawi yathu kumuonetsa kuti zimene amakhulupilila n’zolakwika pamene si zimene iye amakhulupilila . — 1 Akor . 28 Makolo , Thandizani Ana Anu Kukhala na Cikhulupililo Iye analamula Adamu na Hava kuti ‘ adzaze dziko lapansi , ndipo aliyang’anile . . . . Ayang’anilenso colengedwa ciliconse cokwawa padziko lapansi . ’ Anakambanso kuti : “ Kukhala ndi katundu wocepa mu umoyo n’kwabwino kwambili . Bwanji osayamba kuŵelenga Baibo lelo ndi kulola kuti ikuthandizeni kukhala na umoyo wabwino ? Kodi sangateteze anthu abwino ku mavuto amenewa ? ’ NYIMBO : 135 , 139 Izi zitanthauza kuti anthu oposa 90 pa anthu 100 alionse ali ndi Baibulo m’cinenelo cao . Kodi inunso mudzamuyesa Yehova kuti mulandile madalitso ake ? Pa nthawi yovuta imeneyo , Mulungu sanalephele kukomela mtima Rute , amene sanali mwiisiraeli . N’zoona kuti Mabaibulo ena ndi ovuta kuŵelenga ndipo si olondola kwenikweni , koma pafupifupi onse ali ndi uthenga wopatsa ciyembekezo komanso wotsogolela ku moyo wosatha . ( Mateyu 21 : 21 , 22 ) Ena a ife tinasintha khalidwe lathu cakuti anthu amene anali kutidziŵa poyamba amatidabwa . Baibo imamucha kuti “ bwanamkubwa wa kutsidya lina la Mtsinje . ” — Ezara 5 : 3 - 7 . A Daka : Ine ndingakonde . Baibulo limatiuzanso kuti kale , Yehova nthawi zina anali kucilitsa anthu mozizwitsa ndi kuukitsa akufa kudzela mwa aneneli ake . 2 : 12 ) Kaya tili pa nyumba , ku nchito , kusukulu , pa zosangulutsa kapena mu ulaliki , tiyenela kuyesetsa kulemekeza Yehova ndi khalidwe lathu labwino . Tingaphunzile zambili tikaganizila zimene Ahabu anacita . Mwa kucita zimenezi , a Mboni amatsatila citsanzo ca atumwi a Khiristu , amene modzicepetsa anasintha maganizo awo pamene Yesu anawawongolela . — Machitidwe 1 : 6 , 7 . Kodi io anatanthauza ciani ? Conco , m’malo mocedwetsa mwana kubatizika , makolo anzelu amayesetsa kupeleka citsanzo cabwino kwa mwanayo . Ngati tifuna kukhala odzipeleka kwa iye yekha tiyenela kusamala kuti zinthu zina zisakhale patsogolo mu umoyo wathu . Baibulo imati : “ Tate wacifundo cacikulu ndi Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , . . . amatitonthoza m’masautso athu onse . ” — 2 Akorinto 1 : 3 , 4 . Mwadzidzidzi , anaona Yesu akuyenda pa nyanja . ( 1 Akorinto 15 :⁠ 6 ) Mwina panthawiyo m’pamene Yesu analamula ophunzila ake kuti azilalikila “ anthu a mitundu yonse . ” Pamene tikhululukila ena , timaonetsa kuti timayamikila Yehova cifukwa cotikhululukila macimo athu kupitila mu nsembe ya dipo la Khristu . Kaŵilikaŵili limachula za kukhazikitsidwa kwa Ufumu wa Mulungu pansi pa ulamulilo wa Mwana wake , Yesu . Aweluza mlandu mu Khoti Yapamwamba ya Ayuda Khoti Yapamwamba ya Ayuda inali kuweluza nkhani zokhudza malamulo aciyuda . Mwacitsanzo , tingadzamve za anthu ena amene aukitsidwa , ndipo anzao ndi acibale ao akusangalala . ( Gen . 32 : 6 - 12 ) Mwacidziŵikile , iye anali kukhulupilila zimene Yehova anamulonjeza na zimene analonjeza makolo ake , ndipo anali kufuna kucita zinthu mogwilizana na cifunilo ca Mulungu . A Inoki : Mboni za Yehova zili ndi Webusaiti imene ili ndi nkhani zothandiza anthu kukhala ndi mabanja acimwemwe . Lolani Yehova kukutsogolelani , ndipo gwilitsilani nchito malangizo ake a nzelu . ( Ŵelengani Mateyu 13 : 13 - 15 . ) Iye anagwilizanitsa “ kukhala mogwilizana ndi thupi ” na “ zilakolako za ucimo ” zimene “ zinali kugwila nchito m’ziwalo [ zawo . ] ” Nthawi zina , anali kumukakamiza kupita kukaseŵenza ngakhale pamene kwazizila kwambili , ndipo sanali kum’patsa zovala za mphepo . ( Yohane 19 : 20 ; 20 : 16 ; Machitidwe 26 : 14 ) Yesu ayenelanso kuti anali kukamba mau ena a Ciaramu amene anali ofala panthawiyo . [ Mau apansi ] Kuti mudziŵe zambili zokhudza nsembe ya Yesu , onani nkhani 5 mu buku lakuti , Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . [ Cithunzi papeji 6 ] Kudzatithandizanso kuti tizikonda kwambili Yehova , Mlembi wa Baibo amene anatipatsa Mau ake kuti tipindule nawo . — Mika 4 : 2 ; Aroma 15 : 4 . Ponena za anthu amene akuchulidwa m’fanizoli , Yesu ndiye “ Mwana wa munthu , ” kapena kuti Mfumu . Iwo anali kuyembekezela dziko lolonjezedwa “ loyenda mkaka ndi uci . ” M’dzikolo akanapeza mpumulo weni - weni . — Eks . N’nabadwila ku Ukraine mu 1933 , m’mudzi wa Zolotniki . Ni anthu ati amene ali na makhalidwe ochulidwa pa 2 Timoteyo 3 : 2 - 5 ? Iye anakonda coonadi osati cifukwa cakuti amai ake ndi ambuye ake anamuphunzitsa coonadi . 3 : 1 - 3 ) Mwacitsanzo , pakacitika ngozi yacilengedwe anthu amavutika kwambili . Pa cifukwa cimeneci , ndidzakhala ndi mtima womudikila . ” — Maliro 3 : 21 , 24 . KAINI anafunika kupanga cosankha pa nthawi ina . Iye anafunika kusankha kaya kugonjetsa mkwiyo kapena kuulola kumulamulila . Iye ananena kuti pakapita masiku atatu , Farao adzatulutsa wopelekela cikhoyo ndi kumubwezela pa nchito yake yakale . 1 : 13 , 14 ) Mwacionekele , nayenso anadzozedwa pamodzi na ophunzila ena amene analipo . M’fanizo limenelo , anamwali onse anadzuka pamene anamva kufuula usiku kuti : “ Mkwati uja wafika ! ” Safuna kuti uzingotengela cikhulupililo ca ena . N’zokaikitsa kuti kupita patsogolo kwa sayansi kungathandize kutalikitsa moyo wa munthu . Awa sanali maukwati akuti kugonana kunali koletsedwa iyai . Paja Baibo imakamba momveka bwino kuti ‘ mwamuna adzafunika kupeleka kwa mkazi wake mangawa ake . ’ Imakambanso kuti anthu okwatilana sayenela kukanizana pankhani yogonana . Iye anati : “ Ndimakonda lemba la Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . ( Genesis 41 : 1 ) Mwacionekele zimenezi zinamufooketsa kwambili Yosefe . Thandizani Kukongoletsa Paladaiso Wauzimu 2 : 12 ) Makolo akapempha Akhristu ena kuti athandize ana awo , afunika kudziŵa mmene Akhristuwo akuthandizila anawo . Kulikonse kumene ndinali kupita ndinali kunyamula mfuti . Izi zimawalimbikitsa kusintha zikhulupililo zawo , maganizo , na khalidwe lawo . Kukamba zoona , apainiya oyambilila anayenela kulimba mtima ndi kuyesetsa kulimbana ndi mavuto amene anakumana nawo . Buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa Mceni - ceni lili ndi nkhani 19 . ( Akolose 1 : 11 ) Ndipo popeza kuti Yehova amadziŵa bwino cibadwa cathu , maganizo athu , ndi mtima wathu , sadzalola kuti ciyeso cifike pamlingo wakuti sitingakwanitse kupilila . Conco , Faulkner ndi mkazi wake anapita ku msonkhano umene unacitikila ku Twickenham , m’dziko la England m’caka ca 1955 . ( Genesis 13 : 1 - 4 ) Linamanga misasa m’dela la mapili ca kum’mawa kwa Beteli , kapena kuti Luzi , malinga ndi mmene Akanani anali kuchulila . Akatswili pa zankhondo amafalitsa mauthenga abodza kuti afooketse adani awo . Koma kodi amacita bwanji zimenezi ? Cifukwa ciani ? Sitiyenela kulola ‘ dzanja lathu kupuma ’ pa nchito yofesa mbewu za Ufumu . Tikatelo , tidzakhalabe na mwayi wamtengo wapatali wocitila “ umboni ku mitundu yonse . ” ( Mat . Pindulani Mokwanila ndi Cakudya Cakuuzimu Cimene Yehova Amapeleka , May Cinam’thandiza n’ciani ? Baibo imati : “ Ndiyeno Mulungu woona anaona nchito zawo . Anaona kuti alapa ndi kusiya njila zawo zoipa . Motelo , Abulahamu anacita zinthu mwanzelu , ndipo modzicepetsa Sara nayenso anagwilizana nazo . ( b ) M’kupita kwa nthawi , kodi Yehova angagwilitsile nchito bwanji ophunzila okhulupilika ? Iwo anakhalabe okhulupilika ngakhale pa nthawi imene sicinali copepuka kutelo . Koma anapitilizabe kucita zinthu mofatsa ndi moleza mtima mpaka pamene anaphedwa . NYIMBO : 89 , 86 Ndiyeno anaonekelanso kwa abale oposa 500 pa nthawi imodzi , ndipo ambili a io akali ndi moyo mpaka lelo , koma ena anagona mu imfa . ( Luka 2 : 41 - 44 ) Masiku ano , pamene tikuyembekezela moyo wosatha m’dziko latsopano , tifunika kucita zonse zimene tingathe kuti tipitilizebe kukhala ogwilizana . M’kupita kwa nthawi , ambili m’banja la munthuyo anaphunzila coonadi . Kodi kupanduka kwa Satana , Adamu , ndi Hava kunabweletsa mavuto otani padziko lapansi ? Ngati winawake analenga Mulungu , ndiye kuti munthu ameneyo akanakhala Mlengi . Iye amaona anthu amene amacitilidwa mopanda cilungamo . Ndipo amawacitila cifundo ndi kuwathandiza . Kodi nimakhala umoyo wocita cifunilo ca Mulungu mwa Khiristu Yesu ? ’ Inde , nchito yolalikila imatipatsa kapenyedwe kabwino ka zam’tsogolo , ndipo imatilimbikitsa kuti tisatope pa mpikisano wathu wa ku moyo . — 1 Akor . Mzinda wa Betelehemu unali kumwela kwa Yerusalemu . 5 : 27 , 28 ) Koma ganizilaninso citsanzo ca Paulo . Kuphunzila maulosi a m’Baibulo kumatithandiza kudziŵa makhalidwe ocititsa cidwi a Mulungu . ( Machitidwe 10 : 1 - 48 ) Mulungu anatsogolelanso mtumwi Paulo ndi anzake ku mtsinje wina kunja kwa mzinda wa Filipi . Ndinayesanso kufufuza m’Baibulo ya pa intaneti za caka ca “ 1914 . ” Kodi kusintha kumeneku ndi kopindulitsa ? Tidziŵa bwanji kuti Mulungu amatikonda aliyense payekha ? Malemba ambili amanena kuti zinthu zidzakhala bwino kwambili . Iye anauzila amunawo kulemba maganizo ake . Şirin Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi . Yesu anatiphunzitsa kuti ngati tiika maganizo athu pa kukhala ndi zinthu zambili , zingatisokoneze kutumikila Mulungu Baibo imati : “ Anacitadi momwemo . ” — Gen . Gad , mng’ono wake wa Lije anati : “ Tinayenda kwa mawiki angapo ndipo tinali kuona mitembo yambili - mbili . MWACIBADWA munthu aliyense amafuna kukhala paubwenzi ndi ena . Ayuda anali ndi lamulo lakuti ngati cigaŵenga cafa pamtengo umene capacikidwapo , mtembo wake “ usakhale pamtengopo usiku wonse . ” Kodi mfundo imeneyi igwilizana bwanji ndi mfundo yakuti tiyenela kukonda Mulungu ndi mtima wathu wonse , moyo wathu wonse , ndi mphamvu zathu zonse ? Sankhani kutumikila Yehova , ndipo dziŵani zimene iye afuna kuti mucite . N’ciani cingawacititse kufuna kuonelela zithunzi zamalisece zimenezo ? Mateyu 24 : 6 , 7 : “ Mudzamva phokoso la nkhondo ndi mbili za nkhondo . . . . Ine ndabwela kudzacita cifunilo canu . ” Pambuyo pa mlungu umodzi , mtsikanayo anayamba kuphunzila Baibulo , ndipo mosataya nthawi anayamba kusonkhana . ( b ) Nanga n’cifukwa ciani tiyenela kupewa nsanje ndi kudzitama ? Mwinanso mungaganize kuti anali wacikondi , wodekha pokamba ndi pocita zinthu . M’bale wacitatu anati : “ Kukonda zimene Yehova amakonda ndi kudana ndi zimene iye amadana nazo , ndiponso kufunafuna citsogozo cake nthawi zonse ndi kucita zimene zimam’kondweletsa , ndiko kumvela gulu la Yehova . Izi ziphatikizapo kumvela amene iye akugwilitsila nchito kuti akwanilitse colinga cake padziko lapansi . ” Nkhani yaciŵili ifotokoza cifukwa cake cikhulupililo si kumvetsetsa cabe madalitso amene Yehova adzatipatsa . Kodi vutoli linathetsedwa bwanji ? Wamasalimo anakamba kuti : “ Ndi zabwino komanso zosangalatsa kwambili abale akakhala pamodzi mogwilizana ! ” 16 , 17 . ( a ) Tiyenela kucita ciani kuti tikhalebe pa ubwenzi wolimba ndi Yehova ? Mngeloyo anaona kuti ni mwayi wapadela kupeleka uthenga umenewu wocokela kwa Yehova . Sanadzione kuti ni wapamwamba kwambili cakuti sangakambe na munthu wopanda ungwilo . ( b ) Kodi aliyense wa ife angapindule bwanji ndi cisamalilo ca Yehova ? Cotelo , kodi iye anabisa mkanjo wapadela umene anapatsidwa ndi atate ake , abale ake atamuyandikila ? 6 : 7 ) Patapita nthawi , Yesu anafotokozanso pemphelo limeneli koma sanagwilitsile nchito mau amodzimodzi . Noma anati , “ N’nacita cidwi kuona kuti iye analolela kukhala pa kileti . ” Ndipo ngati muli na funso , kumbukilani citsanzo cabwino ca nduna ina ya ku Itiyopiya imene inakhalako zaka 2,000 zapitazo . Kodi omasulila afunika kulemba dzina la Mulungu m’Mabaibulo awo ? Koma kucita mdulidwe pambuyo pa wiki imodzi kunali citetezo cabwino . Kumeneku , iye na mwamuna wake anali kukhala na umoyo wabwino , koma nthawi zina anali kukumana ndi zokhumudwitsa . Iwo anali kunyozedwa ndi kuzunzidwa cifukwa ca makhalidwe ao abwino . TSAMBA 13 • NYIMBO : 83 , 57 Nthawi zambili , Baibo imagaŵidwa m’zigawo ziŵili . Lomba onse akusangalala kutumikila Yehova mogwilizana . Anakhazikitsa kumwamba mozindikila . ” — MIY . Iye anati : “ N’nali kuopa kukakhala ku malo acilendo . Koma Yehova anam’samalila pamodzi ndi banja lake , ndipo anagwila nchito yomasulila mabuku kwa zaka zambili . N’napempha kuti anipatule papulogilamuyo pamaziko akuti n’nali mtumiki wa nthawi zonse , koma khoti inakana pempho langa . Conco , inagamula kuti nikapike jele kwa miyezi 6 . Mu maloto aciŵili analota kuti , dzuŵa , mwezi ndiponso nyenyezi zokwanila 11 zikumugwadila . Ngakhale n’conco , io anapitilizabe kusintha zinthu zina paumoyo kuti akwanilitse colinga cao . Iye anakambanso kuti Mboni za Yehova zilibe abusa amene amalipilidwa . Zimenezi zidzacititsa kuti mucedwe kugaitsa , koma mukanayembekezela pamzela kucigayo coyamba , mukanagaitsa mwamsanga . Abulahamu anagonjela mokhulupilika . — Genesis 21 : 11 - 14 . Kodi mudzakhalabe ndi cikhulupililo cakuti Yehova adziŵa zimenezi ndipo adzacitapo kanthu panthawi yoyenela ? Ndiye cifukwa cake , Baibulo limanena kuti anthufe tili ngati ciwala akatiyelekezela ndi Mlengi Wamkulu . N’cifukwa cake nimalimbikitsidwa ngati anzanga akulila nane . 8 : 20 – 9 : 1 ) Anthu analinso ndi mwai wolambila Mulungu mogwilizana ndi kudzaza dziko lapansi . Tisaiŵale kuti Mulungu anagwilitsila nchito mzimu wake woyela kutsogolela anthu amene analemba Baibulo . ( Aroma 5 : 12 ) Mwakusamvela Mulungu , Adamu anacimwa . Monga takambila m’ndime yapita , mwina Yehova anakwiya cifukwa Mose sanatsatile malangizo atsopano amene anapatsiwa . Tangoganizilani mmene io anasangalalila pamene M’bale Rutherford anakamba nkhani ya mutu wakuti “ Ufumu Wakumwamba Wayandikila , ” ndipo anati : “ Onani , Mfumu yayamba kale kulamulila ndipo inu ndinu atumiki ake olengeza ufumuwo . Iye anali pa nchito yolembedwa . Koma ataŵelenga nkhani ya m’bukulo , anayamba kuganizila zokatumikila ku Myanmar . Pempho yatsopano imeneyi inacititsa kuti apainiya asamatumikile kutali na mipingo , koma akhale m’mipingomo kuti aithandize na kuilimbikitsa . Komabe , ngati mau anu akhumudwitsa ena , bwanji osangopepesa , kukonza zinthu , na kupitiliza kusunga ubwenzi wanu ? Cimene cinakondweletsa kwambili Yehova ndi mzimu wopeleka mofunitsitsa wa anthu amene anacilikiza kulambila koona osati zinthu zimene anapelekazo . Mwa ici , muziyamikila “ mphatso za amuna , ” kapena kuti akulu , amene Yehova wapeleka m’mipingo . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti ndi wacifundo ? Koma anawaona ali patali . ” — AHEB . Koma mwana wa Yefita anapelekedwa monga “ nsembe yopseleza . ” Dzifunseni kuti , ‘ Kodi nkhaniyi ikunicititsa kumvela bwanji ? ( a ) Kodi akapolo aŵili okhulupilika anacita ciani ndi matalente ? Nanga zimenezo zikusonyeza ciani ? Baibulo limaticenjeza kuti sitiyenela kugwilitsa nchito dzikoli mokwanila . M’nthawi ya Nehemiya , Ayuda ambili anali kukwatila akazi omwe sanali kulambila Yehova . Iye anachula za citsanzo coipa ca Solomo . Mtumwi Paulo anati : “ Mukufunika kupilila . ” Pamenepa , tiphunzilapo mfundo yofunika kwambili . ( Mal . 2 : 14 ) Iye amapelekapo maganizo ake mwaulemu pa zosankha zimene zimakhudza banja lao , koma amakhalabe wogonjela . Amaona anthu kukhala ofunika kuposa zinthu Zifukwa zake ni izi . Kuzindikila kumatanthauza kudziŵa cinthu cobisika kapena cosaonekela msanga . ( Aheb . MBILI : MAYI WACICEPELE KOMANSO WOSAMVELA Popeza Mulungu amatidziŵa bwino kwambili , cilango cake nthawi zonse cimakhala coyenelela ndiponso cofunikila . Akuti ngakhale zilombo za kusanga zidzakhala pa mtendele na anthu . ” Cifundo ndiponso zocita zake . Ndi mtima wotani umene muyenela kukhala nao kuti muyenelele maudindo ? Tikatelo , tidzaona kuti mpake Sara kukhala na cikhulupililo cimene anali naco . Muyenela kuimba mokweza monga mmene mumakambila kapena kuposa pamenepo . Mau akuti cilango angatanthauze kutsogolela kapena kuphunzitsa . Ndipo tiwayamikila kwambili pa kudzipeleka kwawo . Motelo tifunika kupitilizabe kuthandiza Akristu anzathu pamene tikuyembekezela nthawi imene sikudzakhalanso ngozi zacilengedwe . ” Yesu , amene io anali kulengeza kuti ndi Mwana wa Mulungu , anali ataphedwa . Cacinai , mwina munali kufuna kuonjezela utumiki wanu , ndipo munaona mmene Yehova anakuthandizilani kukwanilitsa colingaco . Abulahamu , Isaki , ndi Yakobo anali kuyembekezela tsogolo labwino cifukwa cakuti Mulungu anawalonjeza kuti kudzela mwa mbadwa zao , mitundu yonse ya padziko lapansi idzapeza madalitso . Iye ananiwonetsa mau a pa Mlaliki 3 : 6 n’kuniuza kuti pali nthawi “ yovomeleza kuti cinthu catayika . ” Ena angayambe kunyoza zikhulupililo zathu , kutiimba mlandu wakuti tagaŵanitsa banja , kapena kutiopseza kuti adzatikana ngati tipitiliza kucita zimene timakhulupilila . Mwacitsanzo , amaseŵenzetsa nyambo pokopa anthu kuti azicita zofuna zake . 6 : 16 - 19 ) Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Kodi ndiwe womangika kwa mkazi ? Conco , anthu ndi ofunika kwambili kuposa zomela kapena nyama . Kodi Aisiraeli anali kuiweluza bwanji ? Cifukwa ca kusintha kumeneku , anthu anapatsidwa malangizo atsopano akuti : “ Musadye nyama pamodzi ndi magazi ake , amene ndiwo moyo wake . ” Komanso mukamafotokozela Yehova nkhawa zanu kucokela pansi pa mtima , iye amakuyandikilani kwambili . Kodi tumapepala twauthenga tumatithandiza bwanji kugwilitsila nchito Baibulo paulendo woyamba ndi paulendo wobwelelako ? M’Baibo muli zitsanzo zambili za anthu amene Yehova anawacitila zinthu zimene sanali kuyembekezela . Muziona zinthu mmene iye amazionela . Nchito yolalikila uthenga wabwino padziko lonse ndi umboni winanso woonetsa kuti Mulungu amatithandiza . 15 : 6 ) Inde , cioneka kuti ophunzila ambili - mbili a Yesu analipo pamene iye anapeleka lamulo lakuti tiyenela kupanga ophunzila . Kuti mudziŵe za nthawi pamene cilungamo ceni - ceni cidzakhalako padziko lapansi , onani nkhani 3 m’buku iyi , Zimene Baibulo Ingatiphunzitse , yofalitsidwa na Mboni za Yehova Kodi niyenela kuwonjezela nthawi imene nimacita zimenezi ? ’ — Salimo 1 : 2 , 3 . Kuyambila m’caka ca 1920 , misonkhano ya dziko lonse , kapena phwando la bungwe limeneli , lakhala likucitika pambuyo pa zaka zingapo . Timalalikila kulikonse kumene timapeza anthu ( Onani ndime 10 ) Iwo anayankha kuti , “ Buku limene ndinakupatsa lija . ” ( Aheberi 13 : 2 ) Kodi na imwe simungatengele citsanzo cabwino ca Abulahamu na Sara coceleza alendo ? Pa Aisiraeli 10,000 amene anadzipeleka kukamenya nkhondoyo , palibe amene akanakamba kuti ndiye anacititsa kuti apambane . Ni ulosi wolimbikitsa uti umene Yehova anapeleka pambuyo pakuti Adamu na Hava apanduka m’munda wa Edeni ? Kuyambila kale , atumiki okhulupilika a Yehova akhala akuimba nyimbo monga njila yotamandila Yehova . Pofotokoza zimene zinacitika , Peter anati : “ M’rabiyo anadabwa kuti n’nali kuidziŵa yankho , koma ine sin’naone ngati ni funso lovuta . Kanu ndi aka . ” 1 : 13 , 14 ) Popeza kuti Mulungu amatikhululukila macimo , tilinso na mwayi wolandila madalitso ena ambili - mbili . Kodi Tingalimbitse Bwanji Mgwilizano Pakati Pathu ? Iye anali ndi zaka 79 pamene ciyembekezo cake codzaukitsidwa kukhala mmodzi wa abale a Kristu kumwamba cinakwanilitsidwa . — Aheb . Mneneli Yeremiya anali kukonda coonadi ca m’Malemba . Mwamantha , n’nayamba kuyenda kupita kumene iwo anali , ndipo sin’nali kudziŵa kuti nidzakhala na moyo kapena ai . ( Genesis 18 : 20 , 21 ) Panthawi imeneyo , Yehova anasankha kuti asadziŵe mmene kuipa kunaculukila m’mizinda imeneyo . ( b ) N’cifukwa ciani mtsikana wina anasankha kuti asapite ku univesiti ? Koma kodi muona kuti zinthu zidzaipa kufika pati ‘ cisautso cacikulu ’ cisanayambe ? Akufa Adzakhalanso ndi Moyo 8 Mu 2006 Erica , ali ndi zaka 19 , anapita kukatumikila ku Guam . Ndipo zimene iye anakamba zionetsa mmene atumiki acangu amenewa amamvelela . Kendra amene anadwalako matenda a maganizo anadziimba mlandu kwambili cifukwa anali kuona kuti sanali kucita zonse zimene Mulungu amafuna . ( Aroma 12 : 2 ) Ngakhale n’conco , pakali zina zofunika kucita . TSAMBA 24 • NYIMBO : 106 , 49 Conco anasankha kunyalanyaza mau oipa amene anthuwo anakamba . ( Akol . 1 : 6 , 23 ) Mwacitsanzo , mtumwi Paulo atalalikila pa cilumba ca Kupuro , bwanamkubwa wa Roma dzina lake Serigio Paulo , “ anakhala wokhulupilila , pakuti anadabwa kwambili ndi zimene anaphunzila zokhudza Yehova . ” — Ŵelengani Machitidwe 13 : 6 - 12 . Paulo anamvetsetsa mfundo imeneyi . Ali mkati mothaŵa , Sisera anasiya galeta yake podziŵa kuti siingam’pulumutse ndipo anathaŵila ku Zaananimu , dela limene mwina linali pafupi ndi Kedesi . Mwamuna aliyense pakati pa inu azidulidwa . . . kuti ukhale cizindikilo ca pangano la pakati pa ine ndi inu . ” ( Gen . M’malo mwake , anaimba mlandu mkazi wake ndi Mulungu , Mpatsi wacikondi . Pa ulaliki wake wa pa Phili , Yesu anaphunzitsa otsatila ake kupemphela kuti : “ Ufumu wanu ubwele . ” N’cifukwa ciani anthu padziko masiku ano ndi oipa kuposa kale ? Zimenezi zimakhudza malingalilo athu , zokhumba zathu , ndi zinthu zimene timakonda kwambili . Conco , kodi coonadi ca m’Baibo cinasinthidwa ? * Ngakhale kuwapatsa kamphatso kakang’ono monga tayi , kungakhale kothandiza ngako . Nayenso Paulo ayenela kuti anali kukonda Baranaba cifukwa anali wacifundo ndi wokoma mtima . Coyamba , tiyeni tikambilane zina mwa zida zimene tagwilitsila nchito pa zaka 100 zapitazi . DAVIDE wa ku Isiraeli wakale ndi amene anakamba mau amenewa poyamikila mkazi amene anakumana naye . ( Yes . 46 : 10 ) Koma Baibo ionetsa kuti iye amasankha zocitika za kutsogolo zimene afuna kudziŵilatu . ( Gen . Koma Yehova anali atamuona kale . Monga mmene zimakhalila kwa abale ndi alongo ambili amene ali mu utumiki wa nthawi zonse wapadela , ine ndi Angie tinapatsidwa mautumiki atsopano ndiponso ovutilapo . Kodi Kingsley anaphunzila bwanji za Yehova , nanga zinatheka bwanji kuti alembetse m’Sukulu ya Ulaliki ? Zofuna , mikhalidwe ndi thanzi la opeleka cisamalilo zimasiyana . Iye anafunsa atumiki ake m’bwalo la mfumu kuti : ‘ Kodi pangapezekenso munthu wina monga uyu , wokhala ndi mzimu wa Mulungu ? ’ Ndiyeno , mwanayo akayamba kulemekeza makolo ake , adzazindikila kuti akulemekeza Yehova . ( Aef . Mwina aphunzitsi anu ndi ana a sukulu anzanu angavomeleze malingalilo anu . ( b ) Kodi malemba awa : Afilipi 2 : 13 ndi Afilipi 4 : 13 , angathandize bwanji abale kukhala olimba mtima ? Kuti tipilile ziyeso , tifunika kukumbukila kuti pali enanso amene akhala akupilila . ( Mlal . 3 : 12 , 13 ) N’zoona kuti anthufe timakonda zosangulutsa zosiyana - siyana . 4 : 12 ) Ambili a ise tadzionela tekha kuti Baibo ilidi na mphamvu cifukwa yatithandiza kusintha umoyo wathu . N’cifukwa ciani nthawi zina tingaone zinthu molakwika n’kumaganiza kuti munthu wina mumpingo kapena ise , tacitilidwa zinthu zopanda cilungamo ? Amedi ndi Aperisiya anagonjetsa Babulo pamene Mfumu ya Babulo ndi akazembe ake , anali kumwa vinyo m’ziwiya zoyela zimene anatenga m’kacisi ku Yerusalemu , ndi pamene anali kulambila milungu yao yopangidwa ndi anthu . ▪ Yehova Mulungu Amakonda Kukamba ndi Anthu Kodi akulu amene ali m’dela lanu amene ni aang’ono pali inu mumawaona bwanji ? Nanga amene anacokela ku mtundu kapena cikhalidwe cina mumawaona bwanji ? Komanso , aliyense amadzimva kukhala wofunika , wokondedwa , na wotetezeka . Izi ni dyonkho cabe ya madalitso am’tsogolo . ( Sal . ( Onani cithunzi - thunzi kuciyambi kwa nkhani ino ) ( b ) Kodi tiyenela kupewa ciani pamene tigwilitsila nchito Baibulo kuti tione ngati ndife odzikonda ? ( Aroma 12 : 17 , 18 ) Ngakhale kuti Paulo anakumana ndi mavuto ambili , monga “ zoopsa za acifwamba , ” iye anatsatila malangizo amene analemba . Sanaphwanye mfundo za m’Malemba pofuna kudziteteza . ( 2 Akor . Kuti tiyankhe , tiyenela kufufuza Malemba kuti tidziŵe amene adzaukila anthu a Mulungu . Ndipo Baibo imati : “ Mulungu ndiye cikondi . ” Ndipo nthawi zina kupsa mtima kungacititse kuti munthu akhale wovutika maganizo kwa nthawi yaitali . M’zaka pafupifupi 70 zapitazo , anthu akhala akuona kusintha pankhani ya mayendedwe , kulankhulana ndiponso pali zipangizo zina zamakono zimene zapangitsa kuti zacuma zisinthenso kwambili padziko lapansi . 2 : 3 , 4 . Kodi ndimangoyang’ana cabe madalitso amene ndidzalandila m’Paladaiso ? ’ Mau osaiŵalika amenewa anakambidwa ndi mtumwi Paulo ndi Sila kuuza Woyang’anila ndende mumzinda wa Filipi ku Makedoniya . Zimenezi zinalinso ndi maubwino pa nkhani ya umoyo na thanzi . — Numeri 19 : 11 , 19 . Aliyense wa ise ayenela kudzifunsa kuti : ‘ N’ciani cina cimene nifunika kucita kuti nivule umunthu wakale ndi kusauvalanso ? ’ Zimenezi n’zofunika kwambili makamaka ngati m’Baibulo mulibe lamulo lacindunji pankhaniyo . M’bale wina wocokela mu mpingo wathu wa ku Japan anakukila ku Myanmar . Olo kuti tikumane na mavuto aconco , sitiyenela kuganiza kuti Yehova watisiya . ( 2 Timoteyo 3 : 1 , 13 ) Baibulo limakambanso kuti : “ Ine ndikudziŵa bwino , inu Yehova , kuti munthu wocokela kufumbi alibe ulamulilo woongolela njila ya moyo wake . Baibulo silinena cabe za kuukila kwa ‘ Gogi wa Magogi , ’ koma limanenanso za kuukila kwa “ mfumu ya kumpoto ” ndi kuukila kwa “ mafumu a dziko lapansi . ” ( Ezek . 38 : 2 , 10 - 13 ; Dan . 11 : 40 , 44 , 45 ; Rev . N’cimodzimodzi ndi cisoni . M’kupita kwa nthawi cimatha , koma timafunika kucitapo kanthu . Anthu apitilizabe kutsatsa malonda a fodya , ndipo ambili amene ali ndi cizoloŵezi cokoka zimawavuta kuleka . M’kupita kwa nthawi n’naona kuti mau oyamba a m’Baibo , amapeleka yankho lomveka bwino kwambili kuti : ‘ Pa ciyambi , Mulungu analenga kumwamba ndi dziko lapansi . ’ ” — Genesis 1 : 1 . Mkazi wina dzina lake Hee Ran wa ku South Korea anakamba kuti : “ Ndikakhala ndi mavuto aakulu , ndimapemphela ndipo ndikatelo , ndimamva bwino ndipo ndimamva kuti ndili ndi mphamva zopilila mavutowo . ” M’malomwake , anali kuganizila kwambili za unansi wake ndi Yehova . ( Lev . Iwo anali kudzamenyana ndi gulu lankhondo loopsa , anali ocepa komanso analibe zida za nkhondo zokwanila . Nanga tingacite ciani kuti tikule mwauzimu ? Angelo alipo miyanda miyanda yoculuka , mwina amafika m’mabiliyoni ambili . wofesa mbewu amene amagona ? Yesu anakamba kuti ophunzila ake ayenela kulalikila ndi kuphunzitsa uthenga wabwino “ padziko lonse lapansi kumene kuli anthu . ” Kucita zinthu mwanjila imeneyi kudzathandiza abululu anu kuona kuti kutumikila Yehova n’kofunika ngako . Modandaula , amai ake anati , “ Mwana wanga anasiya kundikonda . ” Adzamusamalila bwino kwambili pamene akudwala . ’ ( Salimo 41 : 3 ) Yehova amadziŵa bwino mavuto amene atumiki ake amakumana nao . Iye saiŵala atumiki ake . Baibulo limakamba kuti mumpingo mukhoza kukhala “ abale onyenga ” amene angakambe kuti ndi odzozedwa . Musaleke kucita zinthu zauzimu . Koma Mulungu angadziŵe zenizeni zimene tifunikila ndipo angatipatse zinthuzo cifukwa amadziŵa zonse . Kukamba zoona , Mulungu salekelela zacinyengo . ( 2 Mbiri 20 : 1 , 2 ) N’zolimbikitsa kuti atumiki a Mulungu sanayese kulimbana ndi adani ao mwa mphamvu zao zokha . Pofuna kukuthandizani kupanga zolinga , pa tsamba 308 ndi 309 m’buku la Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa , Buku Lachiwiri , pali mbali imene mungalembepo mayankho a mafunso amene alipo . 43 : 10 - 12 ; 2 Akor . 1 : 12 ) N’zoona kuti io akanalemba uthenga wa Mulungu wopita kwa anthu , koma angelowo saona zinthu monga mmene anthu amazionela . Anali kucita zimenezi mokoma mtima , ndipo anali kuyembekeza nthawi yabwino ndi kupeza malo oyenelela kuti awaongolele . — Maliko 9 : 33 - 37 . N’zacisoni kuti mkazi wanga Jenny , amene anali mnzanga wokhulupilika kwa zaka zoposa 35 , sanaoneko cocitika capadela cimeneci . Nanga zimenezo zikanatheka bwanji ? Kaŵilikaŵili , nyengo imeneyi imaphatikizapo miyezi ya March , April , ndi May Koma ine ndikukuuzani kuti : Pitilizani kukonda adani anu ndi kupemphelela amene akukuzunzani , kuti musonyeze kuti ndinudi ana a Atate wanu wakumwamba . Cifukwa iye amawalitsila dzuwa lake pa anthu oipa ndi abwino , ndi kuvumbitsila mvula anthu olungama ndi osalungama omwe . ” Ngati tiyesetsa kukhala okhulupilika ndi oona mtima polambila , tidzalandila madalitso ambili . Mngelo anawauza kuti , “ Iye sali pano cifukwa wauka kwa akufa . ” ( Mat . Mwamsanga n’namuyankha kuti , “ Ine toto ! ” Eliya anali wamtengo wapatali kwa Mulungu , ndipo Yehova anam’tsimikizila kuti ndi wofunika . Mungacite ciani kuti muthandize anthu amene akukila mu mpingo mwanu ? Mwacitsanzo , Paulo anauza Timoteyo kuti azimwako vinyo pang’ono . Muzikumbukila Atate wanu wamphamvuyonse . Ngati tigwilizana ndi anthu amene samvela malamulo a Mulungu , tingayambe kucita zimene io amacita n’colinga cakuti atikonde . Mwadzidzidzi zinthu zinasintha . Fotokozani . ( b ) N’cifukwa ciani wophunzila Baibo afunika kubatizika kuti akhale Mboni ya Yehova , olo kuti pamene anali ku cipembedzo cina anabatizikapo ? Atapita kukayendela minda yake pa nthawi yokolola , Boazi anaona mkazi wacilendo akukunkha mwakhama m’mbuyo mwa anchito ake . Kodi zimene Asa anacita zinathandiza ? Ikani deti yothela yocikwanilitsila . Zioneka kuti pa nthawiyo Abisalomu mwana wake anafuna kumulanda Ufumu . Ndiyeno anali kuzungulitsa gulaye ndi kuponya mwalawo mwamphamvu kwambili . KODI KULANGA N’CIANI ? Mu Baibulo , liu lakuti ‘ kulanga ’ si mau cabe ena a cilango . Mungacilikize bwanji nchito yomanga Nyumba za Ufumu ? Iye panopa akugwilitsila nchito anthu ake kudziŵikitsa coonadi padziko lonse lapansi . Kodi makolo acikristu angacite ciani kuti aŵete ana ao ? ( 1 Timoteyo 2 : 3 , 4 ) Posacedwapa , Yehova adzagwilitsila nchito Ufumu wake , umene ndi boma la kumwamba lolamulilidwa ndi mwana wake Yesu Kristu , kuononga dongosolo la malonda la umbombo limene limacititsa anthu ambili kukhala akapolo a fodya . Ndipo banjalo limasankha nyimbo zogwilizana ndi nkhani zophunzila tsikulo . ( Ŵelengani Mateyu 13 : 52 . ) Nchito Yomasulila . Ndiyeno anandimanga ndi zingwe n’kundiika m’nyumba imene munali akaidi amene anagwidwa cifukwa ca kuba . Sanaleke kucita cifunilo ca Mulungu . Caciŵili , panthawi imeneyo Atate ndi Amai anacita zilizonse zimene angathe kuti ndisiye kutumikila Yehova . Kucita zimenezi kuli ngati kugwilitsila nchito galasi kuti tione zovala zathu zatsopano koma kulephela kuona zolakwika pankhope yathu . ( Maliko 4 : 24 ) Malangizo a Yehova ndi osavuta kumva ndipo ndi oyenela . Koma tiyenela kusamala ndi kukonzekeletsa mtima wathu kuti tiziwamvela . Yehova adzaloŵelelapo kuti aonetse kuti iye ndi Wolamulila wa Cilengedwe Conse . Koma Yesu anafunika kuyembekezela mpaka pa nthawi yoikika ya Yehova . Mose anadalitsidwa cifukwa ca maganizo ake oyenela . Pamene Mose anaganizila zinthu zimene Yehova anam’citila zaka zonse zimene anam’tumikila , anatsimikiza kuti Yehova amam’kondadi . Mwamuna ndi mkazi m’banja akamatsatila malangizo amenewa amakondana ndi kulemekezana kwambili . YANKHO : Ufumu wa Mulungu ni boma lakumwamba . Malemba amati , Yehova “ amadziŵa anthu ake . ” Paulaliki wake wochuka wa pa phili , Yesu Kristu anati : “ Odala ndi anthu amene ali ofatsa , cifukwa adzalandila dziko lapansi . ” ( b ) Kodi Yehova adzawadalitsa bwanji anthu omvela ? Anthu a Yehova anayamba kale kucita zinthu motsatila mfundo ya pa Aroma 12 : 5 . Lembali limati : “ Aliyense payekha ndi ciwalo ca mnzake . ” Baibo imaphunzitsa kuti Ufumu wa Mulungu Waumesiya , umene ni boma la kumwamba , unayamba kulamulila mu 1914 . Pamene tiphunzila Baibulo , tingacite bwino kupeza mayankho a mafunso awa : ( a ) Ndi mafunso ati amene tiyenela kudzifunsa ? Kodi oyang’anila madela aona kuti m’mipingo yambili muli vuto lotani ? Cofunika kwambili ndi kukhala pamtendele ndi abale anu . 2 : 4 - 7 . Tingalimbane bwanji ndi nkhawa zimenezi ? ( Mateyu 14 : 30 ) Petulo anasiya kuyang’ana Yesu ndipo anayamba kuyang’ana kukula kwa mphepo yamkuntho . Ndipo dziŵani kuti ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse mpaka m’nyengo ya mapeto a nthawi ino . ” Mu 1954 , amishonale amene anali kukhala ku Lahore anakangana kwambili cifukwa cosiyana zibadwa . Izi zinacititsa kuti ofesi ya nthambi iwasinthile m’mautumiki ena . Cacitatu , nthawi zina sitimaona masinthidwe onse amene munthu akupanga . Iye anali munthu wosangalala kwambili cifukwa cakuti anali kucita cifunilo ca Atate wake osati cake . Pelekani zitsanzo . ( b ) N’ciani cingatithandize kumuyandikila Yehova ? Centers for Disease Control and Prevention linati : “ Kupepa fwaka kumabweletsa matenda ndipo kumaononga pafupifupi ziwalo zonse zathupi . ” Komanso anali kukhala m’nthawi yapadela . N’cifukwa ciani mufuna kukhala na cikhulupililo monga ca Marita ? Koma timapewa kunena kuti munthu winawake kapena nkhani inayake imaimila cinacake ca mtsogolo ngati palibe umboni wa m’Malemba wosonyeza zimenezo . Kuthandiza Abale a Kristu Mokhulupilika Kodi Akhristu a m’nthawi ya atumwi anapeleka citsanzo canji pankhani yoimba nyimbo polambila ? N’cifukwa cake mtumwi Paulo analangiza Akhristu kuti ayenela kugonjela atsogoleli a boma monga “ olamulila akuluakulu . ” Mose sanaope zimene Farao akanacita . Mungalandile uthenga wakuti amai kapena atate anu agwa ndi kudzipweteka , adwala matenda a maganizo ndipo acoka panyumba , kapena kuti awapeza ndi matenda aakulu . Munthu atakufunsani kuti kumwamba kuli ciani , mungayankhe bwanji ? “ Iwo anapitiliza kuthandiza anthuwo kumvetsa tanthauzo la zimene anali kuŵelenga . ” — Nehemiya 8 : 1 - 8 . Ndiyeno , n’nauza mnzanga amene n’nali kulalikila naye kuti : “ Nikuona kuti nayamba kuganiza ngati Yona . Pamene iye acezela mpingo adzayesetsa kuwadziŵa bwino abale amene asankhidwa kuti aikidwe pa udindo , ndi kuseŵenza nao mu ulaliki ngati n’kotheka . ( Ŵelengani Luka 10 : 38 - 42 . ) Pamene nthawi inafika yakuti Mwana wa Mulungu abadwe monga munthu , Yehova anasankha namwali wodzicepetsa Mariya , kuti adzakhale mayi wa mwana wapadela ameneyu . “ Akamaŵelenga Baibulo amakhulupilila kuti Mulungu akulankhula nao . A Inoki : Ngati mwamuna nthawi zonse amayesetsa kucita zinthu zoonetsa kuti amakonda mkazi wake , kodi zingakhale zovuta mkazi kumulemekeza ? ( Sal . 83 : 18 ) Kapena pamene munadziŵa kuti mungakhale bwenzi la Yehova . ( Yohane 5 : 28 , 29 ) Yobu adzaona lonjelo limeneli likukwanilitsidwa . Espen ananena kuti : “ Nthawi zambili timapemphela kwa Yehova kuti tisagwele m’mayeselo popeza kuti masiku ano timathela nthawi yocepa pa zinthu za kuuzimu kusiyana ndi kale . Adani amadziŵa kuti ngati msilikali ni wosakhulupilika kwa mtsogoleli wake , sangamenye bwino nkhondo . ( Luka 18 : 29 , 30 ) M’caka ca 1972 , tinadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa . Anthu ena amene tinali kuphunzila nao Baibo anabatizidwa . Zocita zathu . Mu wiki yaciŵili kucokela pamene n’nayamba ulaliki wa ku nyumba na nyumba , n’nakumana na mzimayi wina wa zaka za m’ma 30 . Tinadalila Yehova , ndipo iye sanatisiye . Yehova satipatsa malamulo acindunji pankhani zina . Modzicepetsa anapita kukapepesa kwa m’bale amene anam’khumudwitsa . ( Sal . 90 : 10 ) Mabanja amene samapanga makonzedwe pasadakhale amakakamizika kupanga zosankha mofulumila mavuto akabwela . Mwacitsanzo , Ericka , amene amakhala ku United States , ni dokota . Mu 1950 , munthu wina wa Mboni za Yehova anayamba kuphunzitsa Baibo amayi . 4 : 22 - 29 ) Zoona , Yehova anali ataikilatu tsiku limene adzamasula anthu ake kutatsala zaka zambili kuti zicitike . Iye anati : “ N’naona kuti anthu ambili anali kuninyalanyaza . Ndipo kumeneko Yesu anakumana ndi munthu wina wolemala . ( Yes . 45 : 18 ) Munthu woyamba kulengedwa Adamu anali wangwilo , ndipo Mulungu anam’patsa malo okhalamo okongola , amene ndi munda wa Edeni . 103 : 13 , 14 ) Yesu m’pemphelo lake lacitsanzo anapempha Mulungu kuti : “ Mutikhululukile macimo athu . ” Ngati mukhala wofikilika , mumakhala ngati mwatsegula “ njila ” na kuilambula kuti anthu akhale omasuka kupempha cikhululukilo kwa inu ( Onani palagilafu 4 - 8 ) Makamaka tiyenela kukhulupilila mwana wobadwa yekha Yesu Kristu . Baibo imatiuza kuti tili na ufulu wosankha zimene tingakhulupilile kapena kucita , ndipo zimene timasankha zimakhudza tsogolo lathu . — Yoswa 24 : 15 . Aisiraeli a m’nthawi ya Yesaya anali “ mboni “ za Yehova , ndipo monga gulu anali “ atumiki ” a Mulungu . ( Yes . Umboni wa zimenezi ndi wakuti iye analimba mtima kutsutsa ulamulilo wa Yehova ndi kudzipanga mulungu wolimbana ndi Mlengi . Paja Baibo imati , “ maso owala amapangitsa mtima kusangalala . ” Pambuyo pa zimenezi m’pamene cikwati ca Mfumu cidzacitika . — Sal . Makolo ena amakwanitsa kudzipezela zofunika pamene akhala okha . — Mlal . Nthawi ina , mtumwi Yakobo anafuna kupeleka uphungu wamphamvu kwa Akhristu anzake . Iye watipatsa “ ciliconse cabwino ” kuti atithandize kulalikila . M’macaputa ofotokoza mau a mtumwi Paulo a pa Aroma 5 : 12 , monga m’caputa 6 , timapezamo mfundo zolimbikitsa . Mofanana ndi Yehova , iye anali kuwakonda ndipo anali kuwadela nkhawa cifukwa anali kumwa cabe mkaka , m’malo mwa cakudya cotafuna ca kuuzimu . Abulahamu anamulila Sara mkazi wake N’cimodzimodzi masiku ano . Iye anati : “ N’nazindikila kuti kucita ciwawa sikungathetse zinthu zopanda cilungamo . ( Ŵelengani Nyimbo ya Solomo 4 : 7 , 11 . ) Koma tifunika kusamala kuti tisamaone zosangulutsa monga zinthu zofunika kwambili pa umoyo . Kodi Abulahamu na Sara anafunika kuyembekezela Yehova kwa nthawi yaitali bwanji ? Timakumana ndi masautso cifukwa tikhala m’dziko la Satana . Kucita zambili mu utumiki wa Yehova kudzakuthandizani kukhala na umoyo wokhutilitsa cifukwa mudzakhala na mwayi wolemekeza Mulungu nthawi zonse . Koma cikhulupililo cimene Baibo imakamba , ciphatikizapo zambili . Tidzakambilana zimenezi m’nkhani yotsatila . Kodi nchito yolalikila iyenela kucitika kufikila liti ? Kodi ndili ndi cikhulupililo colimba mwa Yehova ndipo kodi cikondi canga mwa iye cimakula tsiku lililonse ? ’ Zinthu zofunika zimenezi zingaphatikizepo nyumba yabwino , nchito yotithandiza kupeza zosoŵa za banja , ndi nzelu zotithandiza kulimbana ndi matenda . Izi zinali kuphatikizapo kucezela mabanja a Beteli ndi amishonale padziko lonse , kuwalimbikitsa mwauzimu , ndi kupenda mafaelo a ofesi ya nthambi . Panthawi imodzi - modzi , anthu a Yehova akulalikila uthenga wabwino wokamba za Ufumu pa dziko lonse . ( Mat . Marita anatanganidwa ndi nchito zoculuka . ” — LUKA 10 : 39 , 40 . Kodi Yehova amawaona bwanji maboma a anthu ? N’ciani cingathandize ana kuti azimvela makolo awo ? Koyamba na mkango , ndipo kaciŵili na cimbalangondo . N’naonanso mmene mpingo unacilikizila makolo anga mwacikondi . Mwina sitingayesedwe mofanana ndi Aroni ndi banja lake . Mwacionekele , inuyo monga m’busa , mumadziŵa kuti kuphunzitsa ena n’kofunika . N’cifukwa ninji Yesu anati : “ Mudzakhala mboni zanga ” ? Mwacitsanzo , ku dziko lina Mboni zinaikidwa m’ndende popanda kuimbidwa mlandu kukhoti . Zinakhala m’ndendemo zaka pafupifupi 20 . N’cifukwa ciani ? Yesu anayamikila kwambili kuti Marita ndi Mariya anamuitana kunyumba kwao . Kodi kukonda zinthu zakuthupi kumatanthauza ciani ? Cifukwa cakuti anthu a Mulungu amadziŵa kuti kutengela makhalidwe a Yehova n’kwabwino kwambili kuposa dayamondi , golide , kapena zinthu zina za kuthupi . Ena afunika kupitiliza kucita khama kuti azikonda ulaliki . Iye anali Mesiya wa bodza wa m’nthawi imeneyo amene anasoceletsa anthu ambili . 13 : 48 ) Mwacionekele , iwo anadziŵa kuti ubatizo ni wofunika ngako kwa Mkhristu aliyense . Pambuyo pake , abale a Yosefe anapita ku Iguputo kukagula cakudya cifukwa cakuti kwawo kunali njala . Komabe , Yehova sanasinthe . Ena ocepa anali kuyenda - yenda cifukwa kunali kotentha . Kodi vuto limenelo likanathetsedwa bwanji ? 5 : 28 ) Komabe , munthu akhoza kuyamba kudzikonda mosayenela . — w18.01 , peji 23 . Coyamba n’nauzidwa kuti nizitumikila ku Service Department . Ndi nthawi iti yabwino yokambilana ndi anthu ? Misece : Ndi kukamba zinthu zoipa kapena zabodza zokhudza munthu wina , zimene zingaononge mbili yake Yehova angakhumudwe kwambili ngati ise amene watisankha kukhala anthu ake , timayopa kudzidziŵikitsa kwa ena kuti ndise Mboni zake . — Sal . 119 : 46 ; ŵelengani Maliko 8 : 38 . Mwacitsanzo , wamasalimo Davide anakamba kuti Yehova “ amadana kwambili ndi aliyense wokonda ciwawa . ” Iye anakambanso kuti sitiyenela kuyanjana ndi “ anthu obisa umunthu wawo . ” Onani zimene iye analemba m’kalata yake yopita kwa Akhristu a ku Roma pofotokoza mmene anali kuonela Ayuda . Iye anati : “ Cimene ndikufunitsitsa mumtima mwanga ndiponso pembedzelo langa kwa Mulungu ndi lakuti Aisiraeli apulumutsidwe . Muzipempha Yehova kuti akupatseni thandizo kupitila mwa “ mthandizi , amene ndi mzimu woyela . ” Iye anati : “ Ndinaphunzila kusagula zinthu cigulegule . 5 : 14 - 19 . Iye yekha ndiye Mulungu woona , ndipo palibe mulungu wina wolingana naye . Anthu ena akatilakwila , kodi timakwiya kapena kuleka kukambitsana nao ? Makolo anga anali kugwila nchito pa famu , kuyambila m’maŵa mpaka madzulo . ( Ŵelengani Akolose 3 : 21 . ) 2 Akorinto 1 : 21 , 22 ; 2 Petulo 1 : 10 , 11 Ngati mungasankhe kucita zimenezi , mungamve mmene Yury anamvelela atapanga cosankha cokatumikila kumalo amene kukufunika anchito ambili . Iye anati : “ Cimene ndimadandaula naco n’cakuti ndinayamba utumikiwu mocedwa . ” Olo kuti pa nthawiyo anali na zaka 80 , iwo anavomela na mtima wonse ataitaniwa . “ Ndiye cifukwa cake monga mmene ucimo unalowela m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi , ndi imfa kudzela mwa ucimo , imfayo n’kufalikila kwa anthu onse cifukwa onse anacimwa . ” — Aroma 5 : 12 . Ndithu Satana akufuna anthu inu , kuti [ akupepeteni ] ngati tiligu . Tizicitila “ onse zabwino , koma makamaka abale ndi alongo athu m’cikhulupililo . ” ( Agal . Pamene anadya cipatso , Adamu anakana Yehova , ndipo anasankha kudziimila payekha zimene zinabweletsa zotulukapo zovulaza . Tidzaonanso mmene tingalemekezele ufulu wa ena pa zosankha zawo . Uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu ukulalikidwa padziko lonse lapansi , monga mmene Yesu anakambila . Baibulo limatiuza kuti : “ Musamade nkhawa ndi kanthu kalikonse , koma pa ciliconse , mwa pemphelo ndi pembedzelo , pamodzi ndi ciyamiko , zopempha zanu zidziŵike kwa Mulungu . ” — Afilipi 4 : 6 . 6 : 10 ) Patangopita nthawi yocepa , onse anayi anayamba upainiya . Kodi Akristu acikulile amenewa angapindule bwanji ndi uphungu wouzilidwa wopita kwa acinyamata wakuti : “ Kumbukila Mlengi wako Wamkulu ” ? Anati : “ Usacite mantha , pakuti ndili nawe . Usayang’ane uku ndi uku mwamantha , pakuti ine ndine Mulungu wako . Nanga zimene anaphunzitsa zingatithandize bwanji kukhalabe ogwilizana ? ( Aef . 6 : 4 ) Conco , ngati ana anu amalephela kudziletsa , dzipendeni ndi kuona ngati mukupeleka citsanzo cabwino pankhaniyi . Tinalimbikitsidwa ngako ! ” Mmenemo “ adzasangalala ndi mtendele woculuka . ” — Yoh . 10 : 16 ; Sal . Tinakondwela kwambili cakuti tinalila . Anali kukhala mwa dongosolo , mwa mtendele , ndi mogwilizana . — Deut . Ine ndine Yehova . ” — Lev . Nthawi zina ndikafooka kapena kudela nkhawa za tsogolo langa , ndimatenga Baibulo ndi kusinkhasinkha Malemba . ( a ) Kodi timabala zipatso mwa kugwila nchito yanji ? Kumvela makolo anu kuli monga kubweza loni imene munatenga ku banki . Patapita ola limodzi , mtsikanayo anatumiza uthenga kwa mlongoyo pa imelo ndi kumuuza kuti ayamba kuŵelenga bukuli ndipo akufuna kudziŵa zambili . Koma nthawi zina ndi bwino kulankhula . NKHANI YA PACIKUTO | KODI MULUNGU AMACITA NANU CIDWI ? 2 : 22 , 23 ) Ndipo iye amatiyandikila na kutidalitsa potipatsa mtendele wa mumtima . Rabeka anali mkazi wokongola , koma sanali waulesi , zimene zikanacititsa kukongola kwake kukhala kopanda phindu . ( Salimo 146 : 4 ; Mlaliki 9 : 5 ) N’taphunzila zimenezi , n’nayamba kuopa Mulungu pa cifukwa coyenela osati cifukwa coopa kukatenthedwa ku moto wa helo . “ Ndikuyamikila kwambili kuti Yehova ndi Mulungu wanga . ” — Sheryl Ndi kuti kumene Ayuda ambili anali kukhala m’nthawi ya atumwi ? Tizimuyamikila nthawi zonse pa mphatso zimene watipatsa . Mneneli Ezekieli anauzilidwa kufotokoza zimene Gogi wa Magogi adzacita , amene akuimila mgwilizano wa mitundu . Iye analemba kuti : “ Yehova , Ambuye Wamkulu Koposa , wanena kuti , ‘ Pa tsikulo maganizo adzakubwelela mumtima mwako ndipo udzaganiza zocita ciwembu coipa kwambili . Cidzaipa kwambili panthawiyo kukumana ndi mavuto cifukwa cosakhala maso . Mukacita zimenezi Yehova adzakuyanjani . DZIFUFUZENI Pofika mu 1913 , nkhani za M’bale Russell zinali kufalitsidwa m’manyuzipepala 2,000 . Ndipo zinali kuŵelengedwa ndi anthu pafupifupi 15,000,000 . Zinthu zabwino zimene Ufumuwu umacitila nzika zake n’zokhalitsa cifukwa cakuti ulamulilo wake ndi wosatha . 8 : 4 - 8 ) Iye sanafune kucita zimene anthuwo anamuuza cakuti Yehova anacita kumuuza katatu kuti awamvele . Kuleza mtima ni mphatso yocokela kwa Mulungu , ndipo n’kofunika ngako kuti tionetse kuti timam’konda . ( 2 Mbiri 18 : 4 - 6 ) Koma musaiŵale zimene zinamucitikila pamene anayamba kugwilizana ndi Ahabu , amene sanali kukonda Yehova . * Kuwonjezela pa mau na zilembo zeni - zeni za m’Cilamulo ca Mulungu , alembi na Afarisi anali kuona kuti kacigawo ka cilembo ciliconse kanali kofunika maningi . Umenewu unalidi mwayi waukulu . Lemba la Miyambo 18 : 22 limati : “ Kodi munthu wapeza mkazi wabwino ? 2 : 18 . Iye anapitiliza kuti : “ Conco , n’naleka kugwilizana na boma n’kuyamba kucilikiza magulu a anthu ofuna kuti zinthu zisinthe . “ Mwina mungaganize zokamba kuti , ‘ Lomba ndiye pamene ufuna kukamba na ine , koma mzuŵa monse tinali tonse ! ’ Koma kodi Mulungu amatipatsa bwanji cilango ? Zida zina tinazigwilitsila nchito kwa nthawi yocepa , koma zina tikali kuzigwilitsila nchito . Timadziŵa kuti iye ndiye adzatipatsa moyo wosatha . — Luka 12 : 4 , 5 . N’cifukwa ciani ndife otsimikiza mtima kuti sitidzagwilitsidwa mwala ngati tikuyembekezelabe ? Iwo angavomeleze kuti dziko lasintha kwambili kuyambila 1914 , koma amalephela kuona tanthauzo la zimene zikucitikazi . Kodi mungakonde kudziŵa zimene Baibulo limanena ? Pamene Yehova anatuma Mose kukatulutsa anthu ake mu Iguputo , Iye anauza Mose mbali ina ya umunthu wake . Iye anauza Mose mwacindunji tanthauzo la dzina lake . Atatsala pang’ono kuphedwa , Yesu anazindikila kuti ena mwa otsatila ake anali kuyembekezela kuti iye adzakhazikitsa ufumu wake pa dziko lapansi ku Yerusalemu . Anthu ena amakamba kuti zizindikilo za zinthu zakuthambo zimaonetsa mmene khalidwe la munthu lidzakhalila . ( Mlal . 2 : 3 - 11 ) Anthu ambili amene kale anali kuoneka monga otayika , apeza njila ya ku moyo cifukwa ca mphamvu ya Baibo yosintha anthu . Tinawauzanso kuti timalakalaka kuti tonse 4 tikapite kukayenda ku Africa . NDINABADWILA m’mudzi wa Namkumba pafupi ndi mzinda wa Lilongwe ku Malawi mu March , 1930 . Izi zili conco cifukwa cakuti madzi oundana amenewa mwacilengedwe samalola mphamvu ya dzuŵa kulowa pansi pa nyanja . Monga mmene zimakhalila nthawi zambili , yankho linabwela m’njila yosayembekezeka . Pitilizani kusakila ena ambili , musaleke . ” Ndipo m’Baibulo muli malonjezo ambili a Mulungu onena za nthawi ya mtsogolo imene padziko padzakhala mtendele . ” 22 : 37 , 38 ) Nanga tiyenela kucita bwanji tikapemphedwa kupeleka lipoti lathu la utumiki wakumunda ? Yobu sanali kudziŵa kuti n’liti pamene Mulungu adzacita zimenezo . ( Mateyu 6 : 30 - 34 ) Koposa zonse , Yehova adzatipatsa mphatso yamtengo wapatali yomwe ndi moyo wamuyaya cifukwa ca cikhulupililo cathu . — Yohane 3 : 16 . Kuonjezela apo , kuti aweluzidwe mwacilungamo , Paulo ‘ anapempha kuti akaonekele kwa Kaisara . ’ — Mac . ( Mlaliki 7 : 20 ) Koma ngati mufuna kubatizidwa , ndi bwino kudzifufuza kuti muone ngati ndinu wotsimikiza ndi mtima wonse kumvela malamulo a Yehova . MMENE MULUNGU AMAYANKHILA MAPEMPHELO Mulungu amatipatsa zimene tifunikiladi . N’ciani cimayambitsa “ mafunso opusa ndi opanda nzelu ” ? Nanga tingawapewe bwanji ? 11 : 4 ) Conco , Yehova anasiya kukonda Solomo . Umoyo wa banja lathu unakhala wabwino kwambili . Kodi Baibo imati ciani pankhani imeneyi ? Kodi tiyenela kukhulupilika kwa ndani ? N’ciani cidzatithandiza kukhala wofunitsitsa kulalikila uthenga wabwino ? Modzipeleka Sara anacilikiza mwamuna wake pa ulendowu kupita kumalo osadziŵika . Pamene ndinali mwana , ndinali kukhala ndi ambuye anga . Eduardo ndi banja lake anali kupemphela kuti iye apeze nchito imene siiombana ndi ndandanda yake yocita zinthu za kuuzimu . Mulungu Ndi Amene Amakukokani 7 Lemba la Salimo 37 : 4 linanithandiza kucita zimenezi . Lembali limati : ‘ Komanso sangalala mwa Yehova , ndipo adzakupatsa zokhumba za mtima wako . ’ ” Yosefe anali ndi zaka 17 . Kuti ndisamavutike polalikila , ndinagula njinga ya olemala ya mawilo atatu yochova ndi manja . Yesu anakamba kuti tiyenela kukhulupilila onse , Yehova ndi Iye . Lipoti yocokela ku bungwe la UNESCO , inati : ‘ Zikuoneka kuti anthu kuyambila pa 25 miliyoni mpaka 30 anawagwila ndi kuwagulitsa . Tingacite ciani kuti tilimbikitse ena ? Mukali pasukulu , yesetsani kukulitsa luso lolalikila uthenga wabwino . Conco , iye sangaone atumiki ake kukhala osayenelela , cabe cifukwa cakuti alibe maphunzilo a Baibo . — Deut . Ena akandisonkhezela kucita zoipa , kodi ndimamvela Mulungu monga wolamulila kuposa anthu ? Kodi n’zoonadi kuti Mulungu wosaonekayo mungamuone ” ? — Akolose 1 : 15 . Tifunika kuona dzanja la Mulungu pa umoyo wathu . Pamene “ azondi ” aciisiraeli anabwela ku nyumba kwake ku Yeriko , sembe iye anacita mantha ndipo sakanawalandila . Izi zionetsa kuti kuphunzila mmene Yesu anali kuganizila n’kofunika kwambili . Dziko la Australia ndi limodzi mwa maiko amene ali ndi anthu ocepa kwambili padziko lonse , maka - maka kumadela akutali . Mmodzi wa iwo anali Sebina , ndipo pa nthawiyo anali kutumikila monga kalembela . Kukambilana nkhani zimenezi , kudzatithandiza kuona mmene kudzicepetsa ndi kukhululukila ena kumagwilizanilana ndi cilungamo ca Yehova . Kodi n’ciani cingaononge mzimu wathu wodzimana ? Sitikudziŵa ngati Debora mkazi wa Lapidoti anali ndi ana , koma cimene tikudziŵa n’cakuti mau amenewa ndi ophiphilitsa . Kale , kuceleza alendo cinali cinchito . Anthu amene anali kufalitsa ziphunzitso zabodza , anayesa kufooketsa ndi kugaŵanitsa mipingo . ( 1 Yoh . 2 : 18 , 19 ; 2 Yoh . Kwa zaka zoposa 100 , magazini ino yakhala ikuthandiza oŵelenga kudziŵa kuti mapeto ali pafupi . Komabe tikukusungani m’ndende pa zifukwa ziŵili izi : Coyamba , boma likufuna kukutetezani kwa anyamata andale kuti angakupheni . Caciŵili , popeza kuti mumalalikila kuti kudzabwela nkhondo , boma likuopa kuti asilikali adzathawa cifukwa ca nkhondoyo . ” Kodi galamafoni inali yothandiza bwanji ? MMENE BAIBULO INATETEZEKELA : Coyamba , ngakhale kuti okopela Baibulo ena anali osasamala ndi acinyengo , ambili anali aluso ndi osamala kwambili . ( Ŵelengani Yoswa 24 : 15 . ) Cigumula cisanafike , anthu anali kufunika kuseŵenza zolimba kuti apeze cakudya . Kodi iwo sangayamikile ? Iwo anakhala moyang’anana ku mbali ziwili za cigwa cacikulu ca Ela . — 1 Samueli 17 : 1 - 3 , 15 - 19 . Kodi si zimene nanunso mumacita mukalandila kalata yocokela kwa mnzanu kapena wacibale wanu ? N’zovuta kufotokoza mmene tizidzamvelela kuuka tsiku lililonse tili ndi thanzi labwino , mtima uli m’malo , ndiponso tilibe nkhawa iliyonse . Kotsatilapo kanali kapepala ka Uthenga wa Ufumu Na . 30 , kamene kanatulutsidwila pamodzi ndi kacingelezi . Tikamamukonda kwambili Mulungu , iyenso amayamba kutikonda kwambili , ndipo ubwenzi wathu ndi iye umalimba . — Ŵelengani 1 Akorinto 8 : 3 . Ganizilani kulimba mtima kumene Yosefe anaonetsa pamene mkazi wa Potifara anamunyengelela kuti acite naye ciwelewele . Sisera anafuna kuphelatu gulu la nkhondo la Aisiraeli mwamsanga ndi mosavuta monga mmene zimakhalila pokolola balele . Satana anacita izi m’njila yakuti zioneke ngati kuti Mulungu ndiye anacititsa mavuto a Yobu . Ngakhale Akhristu amene anabatizika ali aakulu , amakumana na ziyeso zambili zimene sanali kuyembekezela . M’munda wa Edeni mmene anthu anayambila , Mlengi anauza munthu woyamba Adamu kuti : “ Zipatso za mtengo uliwonse wa m’mundamu uzidya ndithu . Muzichula zinthu mwacindunji m’pemphelo lanu . Kodi ‘ makhalidwe oyela ’ n’ciani ? ( 2 Mbiri 20 : 20 , 29 ) Mwacitsanzo , ganizilani mmene Yehova anapulumutsila anthu ake pa Nyanja Yofiila pamene anali kuthamangitsidwa na asilikali amphamvu a Farao . ( Eks . 14 : 21 - 30 ; Sal . Abale ndi alongo padziko lonse amavomeleza mfundo yakuti kukwatiwa “ mwa Ambuye ” ndi kwabwino . Kunena mwacidule , yankho ndi lakuti sitidziŵa . 55 : 13 ) Zoona , ni “ mphatso ya Mulungu ” kuti ‘ tizapulumutsidwa kudzela m’cikhulupililo . ’ Patapita mlungu umodzi titasamukila ku Germany , atate anadwala sitoloko ndipo anakomoka . Yesu anafuna kutithandiza kudziŵa kuti Yehova ndi amene amapangitsa coonadi kukula m’mitima ya anthu a “ maganizo abwino . ” ( Mac . 13 : 48 ; 1 Akor . 15 : 3 , 5 . Kuti tiyankhe funso lofunika limeneli , tiyeni tikambilane mafanizo aŵili a Yesu okamba za kufunika ‘ kobala zipatso . ’ ( Mat . Ophunzilawo anali kugwilitsila nchito lamulo la Aroma pofuna kuteteza uthenga wabwino . — 2 / 15 , masamba 20 - 23 . Koma io amayenda mtunda wamakilomita angapo mlungu uliwonse kucoka kumudzi kubwela kutauni kudzasonkhana . Lana atawafotokozela mmene zinthu zinalili , a Elke , amai a mnzakeyo anamutenga n’kupita naye kunyumba kwao . ( Aheberi 12 : 1 ) Mwa kumvela Mlengi wawo , iwo amaonetsa kuti asankha Mulungu kukhala Atate wawo ndiponso wowaumba osati Satana . Ena a ife takhala tikulimbana ndi adani amenewa kwa zaka zambili . 40 : 1 - 16 . Pa kutha kwa nthawi zokwanila 7 , Mulungu anali kudzakhazikitsa wolamulila watsopano wakumwamba kuti akhale woimila ulamulilo wake . Fotokozani kusiyana pakati pa kudzipeleka ndi ubatizo . 9 : 1 - 5 ) Ena mwa anthu ocepa amene anapulumuka anali Yeremiya , Baruki , Ebedi - meleki , na Arekabu . Mosiyana ndi wamalonda uja , munthu ameneyu sanali kufunafuna cuma . N’CIFUKWA CIANI tiyenela kuwonjezela zimene timacita polimbikitsa ena ? Kodi pali mfundo imene inakulimbikitsani pamisonkhano ? Onani kuti wokwela pa hosi yoyamba , Yesu , anayamba ulendo wake pamene anapatsidwa cisoti cacifumu . 35 : 18 . Kukamba zoona , ngati anthufe sitilimbikitsana umoyo umakhala wovuta . 28 : 19 , 20 ) Imeneyi si nchito yopepuka , ili na zovuta zambili . M’Baibo , kudzicepetsa kumatanthauza kupewa mzimu wonyada ndi mwano . Koma akasinkhuka , samakamba zambili na makolo awo . Tingagwilitsile nchito bwanji pemphelo lopezeka pa Mateyu 6 : 9 - 13 mu ulaliki ? Yehova adzapatsa anthu ambili mwai wokhala ndi moyo wosatha padziko lapansi , ndipo ena adzakhala ndi moyo kumwamba kuti adzalamulile ndi Yesu . Mavuto amene timakumana nao masiku ano , angakhale ofooketsa ndi opweteka , koma tisaiŵale kuti ndi akanthawi cabe . Nthawi zambili io amatumizidwa kumadela osoŵa . Woyang’anila dela amatumikila mipingo ingapo . Tidziŵa kuti nchitoyi imatheka kokha cifukwa ca thandizo la Yehova . — Yobu 42 : 2 . Ai . Kucita zimenezo kukanapangitsa kuti Yehova asawateteze . — 1 Akor . Patapita zaka zocepa , iye analakwitsa zinazake ndipo cikumbumtima cake cinayamba kumuvutitsa . 2 : 16 , 17 ) Kwa Adamu ndi Hava , lamulo limeneli linali losavuta kulimvetsetsa kapena kulitsatila . Munalibe cidani kapena anthu ozunza anzawo cifukwa ca cipembedzo , zinthu zimene zinali zofala m’nthawi ya Inoki . Mu 1914 , kwa nthawi yoyamba , padziko panabuka nkhondo imene inakhudza maiko onse . Ngati Yehova anathandiza Yobu kukhalanso pa mtendele ndi anzake atatu aja , cingam’letse n’ciani kundithandiza kuti ndikhalenso pa mtendele ndi akulu ? ” — Yobu 42 : 7 - 9 . ( Mlal . 7 : 7 ) M’malo mowaimba mlandu , tiyenela kucita nawo zinthu mozindikila ndi mwacifundo . Ŵelengani Yesaya 32 : 1 , 2 . Kale , n’nali kungopezeka pa misonkhano koma osayankhapo , poganiza kuti palibe aliyense amene angamvetsele zokamba zanga . M’salimo limeneli , iye anati : “ Koma ine ndakhulupilila kukoma mtima kwanu kosatha . Kodi ni mphatso iti yapadela imene Mulungu anatipatsa ? ( b ) Kodi tiyenela kutsimikiza mtima kucita ciani ? ( Afilipi 4 : 7 ) Ngati tiuza Atate wathu wakumwamba nkhawa zathu , tidzakhala ndi mtendele wa m’mganizo . ( b ) Kodi mfundo za Yehova na cikumbumtima cathu zimagwilizana bwanji ? 12 Acinyamata ​ — Kodi Mungakonzekele Bwanji Ubatizo ? Anayang’ana za kutsogolo na kucita zinthu mwanzelu . Koma Ramoni anatsala ku Zaragoza . Kukamba zoona , anthu alephela kuthetsa upandu . Cifukwa cakuti Yehova analosela za kuukilidwa kwa anthu ake . Ndiyeno , mtengo wansembe yake unafunikila kupelekedwa kwa Yehova kumwamba . Katswili winanso anakamba kuti cifukwa cotsatila mauthenga osoceletsa , amuna ndi akazi ambili “ asoceletsedwa mosavuta mpaka kufika pocita zinthu zoipitsitsa , ” monga ‘ kupulula mtundu wathunthu wa anthu , nkhondo , kudana cifukwa cosiyana mitundu ndi zipembedzo , ndiponso makhalidwe ena oipitsitsa . ’ — Easily Led — A History of Propaganda . Tinaona cikondi ca Yehova , Mulungu wathu wokhulupilika , ca ana athu , ndi ca anthu ambili amene tinawathandiza kuphunzila coonadi . Araceli : Panthawi imeneyo , ndinali ndi zaka 14 , Lauri anali ndi zaka 12 , ndipo Ramoni anali ndi zaka 10 . Iye angagwilitsile nchito cizunzo ca mwacindunji kapena ca mwakabisila kuti atifooketse . Kumatithandiza kudziŵa kuti ngati takumana ndi mavuto , si ndiye kuti Yehova watikwiyila , koma zimatipatsa mwayi woonetsa kuti timacilikiza ucifumu wa Mulungu . ( Miy . Koma Ufumu wa Mulungu ndi umene ungakwanitse ndipo udzacitadi zimenezi . Colinga cathu ndi kusamalila makolo athu tsiku lililonse mmene tingathele kuti akhale otetezeka . M’nkhani ino , tikambilana zimene ena m’nthawi ya atumwi anacita kuti atumikile Yehova . Zimene taphunzila m’masophenya amenewa zatithandiza kukhulupilila kuti Yehova sadzawononga anthu olungama pamodzi ndi oipa . Mofanana ndi Aisiraeli amene sanali kukwanitsa kupeleka nsembe zodula kwambili , atumiki a Yehova okondedwa amene sangakwanitse kucita zambili , naonso angapeleke lipoti . Kodi cidzacitika n’ciani ? Anthu ambili aona kuti kukhala wowoloŵa manja kumawathandiza kukhala olimba mwauzimu . — Sal . Conco , tingathe kuona kuti Inoki anakhala na banja ali na zaka pafupi - fupi 65 . 28 : 20 ) Komabe anthu amene analeka kugwilizana ndi gulu la nkhosa la Mulungu , kapena kuti amene anadzilekanitsa ndi gulu , n’zokaikitsa kuti adzapulumuka . — Mika 2 : 12 . Kodi nkhani ya woyang’anila ndende igwilizana bwanji na nchito yathu yolalikila ? ( b ) Nanga ndi anthu ati amene Yesu anaukitsa ? Muzicilikiza ulamulilo wa Mulungu popanga zosankha ndi pocita zinthu m’banja ( Onani palagilafu 16 - 18 ) Kuti mulipeze , mufunika kusakila mwakhama . . . . Yehova anali kupatsa Adamu na Hava zonse zofunikila pamene anali m’munda wa Edeni . N’cifukwa ciani nchito imeneyi ikuyenda bwino kwambili ? Mwacionekele , pamene mbusayo anauza mtsikanayo kuti “ ndiwe wokongola paliponse , . . . ndipo mwa iwe mulibe cilema ciliconse , ” sanali kutanthauza maonekedwe akunja cabe . Colinga cathu pamene tilalikila , ni kulemekeza Yehova . Cikondi monga cimeneci “ cimapilila zinthu zonse ” m’lingalilo lakuti cimathandiza okwatilana kutsiliza mavuto na kupitiliza kukhala ogwilizana ndi amtendele . Kodi mukukumbukila zimene zinacitika ? N’zoona kuti mwina tidzakumana ndi mayeselo . Kuti atithandize kukhala na cikhulupililo colimba , Yehova watipatsa ciani mokoma mtima ? Nanga tifunika kucita nazo bwanji ? 3 : 19 . 2 : 3 ) Kodi inu mudzatengela citsanzo ca Yehova mwa kukhala odzicepetsa ? Patapita nthawi , iye anazindikila kuti maseŵelawo anali aciwawa ndi oika moyo pa ciopsezo . Onani Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 , tsamba 28 mpaka 29 , ndime 12 . Ndipo tingaonetse kukhulupilika mwa kuphunzila kucita zinthu mogwilizana ndi atumiki ake odzipeleka , amene iye amawakonda olo kuti amalakwitsa zinthu zina . Mwina pali anthu amene akukucitilani zinthu zoipa , kukupatulani , kapena kukunyozani . Monga mmene zinalili kwa Davide , Yehova sanasiye Rute ndi Naomi . Mzimu woyela unathandiza Mose kucita zozizwitsa ndi kulengeza dzina la Mulungu kwa Farao . Mulungu afuna kuti tikhale mabwenzi ake . — Yakobo 4 : 8 . ( Salimo 37 : 11 ; 72 : 14 ) Kodi simungafune kudziŵa zimene mungacite kuti muyenelele kudzakhala m’dziko lopanda nkhanza ? ( Yakobo 1 : 5 , 6 ; Yuda 22 , 23 ) Sitiyenela kudabwa ngati anthu amatinenela mabodza . Ndipo ngati mukuŵelenga izi , dziŵani kuti ine kulibenso . Mulungu anawacotsa mu Edeni , ndipo analibe ciyembekezo cobwelelanso . Amene ayenela kudya zizindikilo za pa Cikumbutso ndi okhawo amene mzimu wawacitila umboni kuti ndi ana a Mulungu . Kodi Akristu ofikapo ndi osiyanasiyana bwanji ? Nanga ndi ofanana pa ciani ? ( Mat . 24 : 22 ) Tsopano io anali ndi mwai womvela malangizo a Yesu . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana zocitika zina ziŵili zoonetsa kupanda cilungamo kumene kunacitika pakati pa anthu a Yehova m’nthawi yakale . Kodi kudziŵa zimenezi sikuyenela kutipangitsa kugonjela ndi kuyandikila Mfumu yathu ? Mtumwi Paulo anafuna kuti Akristu a ku Efeso akhale ofikapo kuuzimu . Koma kodi zipatso zimene mmela wa tiligu umabala n’ciani ? Kodi kuganiza monga Khristu kumatithandiza bwanji ? Funso lina lofunika kwambili n’lakuti : ‘ Kodi m’baleyu ali na makhalidwe ati abwino amene ningatengeleko ? ’ Nthawi yakuti msonkhano uyambe yatsala pang’ono kukwana . ( Genesis 1 : 12 ) M’kupita kwa nthawi analenganso zinthu zina zofunika kwambili pa umoyo . Kodi zimenezi zimatikhudza bwanji ? Munthu aliyense angadwale matenda osacilitsika pa nthawi iliyonse . Mfundo yakuti ticititse ziwalo za thupi kukhala “ zakufa ” ikusonyeza kuti khama ndi lofunika kuti tipewe zikhumbo zoipa . Kodi anthu a Yehova ndani masiku ano ? Nanga a “ nkhosa zina ” afunika kucitanji kuti akatetezedwe pa “ cisautso cacikulu ” ? Dziŵani kuti Yehova amayamikila zoyesetsa zathu pomutumikila . Wacibale kapena bwenzi lathu lapamtima , mosayembekezela angafunike kusankha kaya kuikidwa magazi kapena ai . Ganizilani mmene mungapindulile ngati muonetsa makhalidwe amenewa . ( Sal . 40 : 5 ) Komanso , mapemphelo athu ayenela kuonetsa kuti ‘ timakumbukila amene ali m’ndende ngati kuti tamangidwa nawo pamodzi . ’ ( Dan . 9 : 25 ) Pomaliza , Yesu Khiristu anadziziŵikitsa kuti ndi “ Mtsogoleli ” wa anthu a Mulungu . Tingatengele bwanji cikhulupililo ca Nowa ? Mwina iye sadzaonanso banja lake . Zaka ziŵili m’mbuyomo , Yesu anali atalamula atumwi ake kuti : “ Pitani ndi kulalikila kuti , ‘ Ufumu wakumwamba wayandikila . ’ ” ( Mat . Amene amalambila Mulungu afunika kukhulupilila zinthu zofanana . — 1 Akorinto 1 : 10 , 11 . ( 1 Tim . 3 : 6 ) Koma n’zomvetsa cisoni kuti ngakhale atumiki ena a Yehova anagwela mu msampha wa kudzikweza . Cinanso , anayamba kusamalila udindo wake monga mutu wa banja . Izi zinakondweletsa mkazi wake ndi ana . ” — Luka 6 : 41 , 42 ; Yak . Elias Hutter anabadwa mu 1553 , m’tauni yaing’ono yochedwa Görlitz m’dziko la Germany . Tauni imeneyi ili kufupi ndi malile a maiko a Poland na Czech Republic . Kale , tinali kuona kuti zimenezi sizingatheke . Kodi pali acikulile amene anapindula ndi nkhani imeneyo ? Si zokhazo , Yehova wanidalitsa mwa kunipatsa banja — cinthu cimene n’nasoŵeka pamene n’nali kukula . Onani zimene Yesu anakamba pa lembali . Kodi Mkhiristu angayambe bwanji ‘ kuika maganizo ake pa zinthu za thupi ’ ? Ndithudi , Yobu anali munthu wosiyana ngako ndi anthu ambili olemekezeka na olemela a m’dzikoli ! Koma kumbukilani kuti pamene munadzipeleka kwa Yehova na kubatizika , munaonetsa kuti mwapanga ubwenzi wapadela na iye . Mau amenewa amafotokoza bwino mtima woipa umene Satana ali nao . Taganizilani citsanzo camakono ici : Joachim anabatizidwa mu 1955 , koma mu 1978 anacotsedwa mumpingo . Atsogoleli acipembedzo anacilikiza nkhondo ndi mtima wonse . Nimalimbikitsidwa kudziŵa kuti anthu ambili anali kumukonda Arthur . Mtambo wakuda unawonekela modabwitsa . Zimenezi zikugwilizana ndi mau a m’Baibulo akuti : “ Munthu amene akuyenda alibe ulamulilo wowongolela mapazi ake . ” — Yeremiya 10 : 23 . Anatsatilanso malangizo amene Akristu anzake anam’patsa . Magazi a nyama anali umboni wa pangano la Cilamulo , pamene magazi okhetsedwa a Yesu ndi umboni wa pangano latsopano . Kodi cikanakhala bwino kuti anthu azidzilamulila okha ? ( Gen . Ngati anthu a m’gawo lanu akuvutika cifukwa ca tsoka lacilengedwe limene linacitika posacedwapa , mungayambe ulaliki wanu mwa kunena kuti : “ Nabwela pano kuti titonthozane . Alendo anafunika kudya ndi kugona ku mahotela , koma kunafika alendo ambili kuposa amene anali kuyembekezela . Tiyelekezele tele : Ambili a ife timasangalala kudya zakudya zonzuna nthawi na nthawi . Koma timadziŵa kuti kudya kaŵili - kaŵili zakudya zonzuna monga makeke , cokoleti , mabisiketi , ndi zina zaconco kungawononge thanzi lathu . Iye sanakopeke na ziwanda zimene zinavala matupi a anthu . Ziwanda zimenezo ziyenela kuti zinali kucita zinthu zodabwitsa pofuna kukopa anthu opanda cikhulupililo ndi otengeka - tengeka . Ni madalitso ati amene muyembekezela mwacidwi ? M’maiko ena , amagwilitsila nchito njila zambili zocilitsila matenda . 102 : 3 , 4 , 6 , 11 ) Iye anaona kuti Yehova afuna kumutaya . — Sal . Mwacitsanzo , mbale wina amene anali atacotsedwa kwa zaka 25 anati : “ Kucokela pamene ndinabwezeletsedwa mumpingo , cimwemwe canga cikungoonjezeleka cifukwa ndakhala ndikulandila ‘ nyengo zotsitsimutsa kucokela kwa Yehova . ’ ( Mac . 4 : 2 . N’cifukwa ciani Yosefe anali kuwaopa Ayuda ? Mukamaceza nao , adzakuthandizani kupanga zosankha mwanzelu ndi kukhala Mkristu wofikapo . — Ŵelengani Aheberi 5 : 14 . N’zitsanzo ziti za m’Baibo zimene zionetsa kuti kudziletsa n’kofunika ? Safuna kuti aliyense akawonongedwe . Ngakhale kuti anthu a m’gawo lake analibe cidwi kwambili ndi uthenga wa Ufumu , iye anali wakhama mu ulaliki . Iye analimbikitsa otsatila ake amene adzakhala ndi moyo m’masiku otsiliza kuti ayenela kukhala maso pamene anati : “ Simukudziŵa tsiku limene Ambuye wanu adzabwele , ” ndipo “ pa ola limene simukuliganizila , Mwana wa munthu adzabwela . ” ( Mat . Akatswili amanena kuti ngati anthu apitilizabe kukoka fodya , podzafika mu 2030 ciŵelengelo ca anthu amene amafa caka ndi caka , cidzaonjezeka kuposa pa 8 miliyoni . Yankho tikulipeza m’fanizo la Yesu . Conco , m’Rabi wina wake akaona munthu wakhate mumzinda , anali kumuponya miyala ndi kumuuza kuti : “ Pita ku malo ako , usadetse anthu kuno . ” Yehova watiphunzitsa zambili zokhudza Yesu kuti titsatile bwino mapazi ake . — 1 Pet . Tifunika kukhala osiyana ndi dongosolo loipali limene tikukhalamo . Pali abale ndi alongo okhulupilika mamiliyoni ambili amene tingasankhe kuti akhale anzathu . Patapita zaka 17 , pambuyo pa ngozi imene inacitikila Sidnei , amene tamuchula kuciyambi kwa nkhani ino , iye anakamba kuti : “ Sindinaimbe Yehova Mulungu mlandu cifukwa ca ngozi imene inandicitikila , koma n’zoona kuti poyamba ndinakhumudwa ndi iye . Kukhulupilila kuti Yesu anauka kumatilimbikitsa kucita cifunilo ca Mulungu . Acita zimenezi cifukwa cakuti afuna kucita zambili potumikila Yehova . Anali azimulamu anga , ndipo anali a Mboni za Yehova . Madalitso a Mulungu amaphatikizapo zambili osati cabe kukhala naye paubwenzi . Iye amatitsimikizila kuti adzatipatsa zonse zimene timafunikiladi . ( Oweruza 11 : 32 , 33 ) Koma kodi Yefita anapeleka ndani kwa Yehova ? Conco , iye sangalekelele khalidwe loipa . ( Hab . N’ciani cinathandiza Yesu kucita zimenezo ? Mungacite phunzilo limeneli panthawi ndi malo amene mufuna . Iye amawononga anthu oipa ngati palibe mwina mocitila . — Ezekieli 18 : 32 . Nanga masomphenya amenewa a m’buku la Zekariya atikhudza bwanji ise masiku ano ? Anati anthu angathe bwanji mantha na kuyamba kukaikila zimene akuwaphunzitsa ! ( Sal . 86 : 3 ) Ngati timakhala na nthawi yokwanila yomuuza Yehova za mumtima mwathu , timayandikila kwambili kwa Atate wathu wakumwamba , amene ni “ Wakumva pemphelo . ” ( Sal . Tikamawelenga ndi kusinkha - sinkha zimene zinacitikila abale athu ndiponso nkhani za m’Buku Lapacaka , timalimbikitsa cikhulupililo cathu mwa Yehova amene ndi pothawilapo pathu . Ndipo n’cifukwa ciani ? Popeza kuti ndinu wacikulile , mosakaikila mumadziŵa zinthu zambili . Kodi Mukuyesetsa Kufika pa Ucikulile Umene Kristu Anafikapo ? Odzozedwa ndi okonzeka kukwanilitsa utumiki wao mpaka mapeto . A Zulu : Buku la m’Baibulo la Danieli limafotokoza za nkhani yaikulu imeneyi nthawi zambili . Ulosi wocititsa cidwi umenewu ni umodzi mwa maulosi ambili opezeka m’Baibo amene anakwanilitsidwa mosalephela olo pang’ono . Msilikali waciroma ngati sanavale nsapato , ndiye kuti sanali wokonzeka kumenya nkhondo . 5 : 22 , 23 ) Mfundo imeneyi siitanthauza kuti mkazi ni munthu wotsikilapo kwa mwamuna iyai . N’nali Kuopa Imfa ( Y . Conco , mwana akangobadwa , makolo afunika kukhala na colinga com’thandiza kuti adzakhale wophunzila wa Khristu kapena kuti mtumiki wa Yehova , wodzipeleka na wobatizika . Lemba la Yohane 3 : 16 limanenanso kuti Mulungu anaonetsa cikondi cake mwa kutumiza Yesu , Mwana wake , padziko lapansi kuti adzatiphunzitse za Mulungu , Atate ake , ndi kudzatifela . Abale na alongo oculuka padziko lonse amatipemphelela . ” 4 : 13 , 16 ) Panthawiyo , Timoteyo anali kale mlaliki wa Ufumu wacangu . ( Yoh . 18 : 10 ) Koma Yesu anauza Petulo kuti : “ Bwezela lupanga lako m’cimake , pakuti onse ogwila lupanga adzafa ndi lupanga . ” N’cifukwa ciani tiyenela kulemekeza zosankha za ena ? Muzitengela Yesu pankhani yosankha mabwenzi . Pambuyo pa msonkhanowo , n’nabwelela kukatumikila ku Philippines . Yesu sanatengeko mbali m’mikangano ya ndale imene imagaŵanitsa anthu . Kodi acibululu osakhulupilila tizikamba nawo bwanji ? Makolo anga naonso anayesa kutiletsa kugwilizana ndi a Mboni . ( 1 Pet . 5 : 8 ) Dziŵani kuti m’bale angakhudzidwe kwambili ndi Malemba osankhidwa bwino amene mungaŵelenge naye . — Ŵelengani Aheberi 4 : 12 . ( Sal . 27 : 10 ) Conco , pa mavuto aliwonse amene mungakumane nawo , pemphani Yehova kuti akupatseni mphamvu na kukuthandizani kucita zinthu mogwilizana na kudzipeleka kwanu . — Ŵelengani Afilipi 4 : 11 - 13 . Pamene Aisiraeli anaona tunthu tumenetu kwa nthawi yoyamba anafunsa kuti : “ N’ciani ici ? ” Kodi umapatula nthawi yoŵelenga nkhani zimenezi ? Iwo afika pakuti angaononge ndi kuseselatu anthu padzikoli cifukwa ca zida zankhondo zimene ali nazo . Kodi mphatso imeneyi ingatithandize bwanji kutsanzila Yehova ? Mwanda umodzi ni 10,000 . Ndinayamba kupezeka pa misonkhano ku Nyumba ya Ufumu pa Sondo . ( b ) Nanga tingacite bwanji zimenezi ? Baibulo limatiuza kuti Mulungu waika nthawi imene mapeto adzafika . ( Machitidwe 1 : 8 ) Kodi io akanakwanitsa bwanji kulalikila padziko lonse lapansi ? Tsiku lina , munthu wina anabwela ku Nyumba ya Ufumu ina m’dziko la Switzerland ndi kunena kuti afuna kukhala wa Mboni . Takambilana zinthu zocepa cabe za mmene pemphelo lingakuthandizileni . M’zaka za m’ma 1520 , Lefèvre anamasulila Baibo m’Cifulenci kuti athandize anthu wamba kulimvetsetsa . Kufunsa mafunso mwaluso kungatithandizenso kudziŵa cifukwa cake womvela wathu amakhulupilila nkhani inayake . Mwa kutipatsa mtendele wa maganizo umene ungatikhazike mtima pansi na kucepetsa nkhawa . Ni mbali ziti zimene tingafunike kugonjetsa kuti tipeze madalitso a Mulungu ? Zimenezi zinali zosangalatsa kwambili . Kudzicepetsa ndiye kunathandiza Barizilai kupanga cosankha canzelu . Pa zaka zocepa zimene tinakhala ku New York City , misonkhano ingapo yacigawo inacitikila ku Yankee Stadium . Izi zionetsa kuti cikumbumtima cawo cinali kuwavutitsa . Onani zimene wacicepele wina dzina lake Carissa anakamba ponena za mmene Kulambila kwa Pabanja kwapindulitsila banja lao . Mwacitsanzo , zaka zapitazo , mnyamata wina ku Europe anayamba kupezeka pa misonkhano yacikhristu . Kodi mumaonetsa bwanji kuti mumakonda ana anu mukamawaphunzitsa kucita zinthu zimene timacita nthawi zonse potumikila Yehova ? 4 : 9 ) N’cifukwa ciani kucelezana n’kofunika ngako masiku ano ? Nthawi zambili wodwala akakhala pafupi kumwalila , amaonetsa zina mwa zizindikilo zotsatilazi , kapena zonse * : Atate anatilonjeza kuti sadzatisiyanso , ndipo sanatisiyedi . Mukayenda mwamsanga , nayenso ayenda mwamsanga . Yehova watiuza zimene tifunika kucita kuti tikhale mabwenzi ake . Zioneka kuti kale anthu ambili a ku Lusitara anali kukhulupilila kuti milungu yao imadzisandutsa anthu . Nanga kuukitsidwa kwa Yesu kumatanthauza ciani kwa inu ? ( Luka 16 : 9 ) Idzafotokozanso mmene tingapewele kukhala akapolo kwa anthu amalonda m’dzikoli , komanso zimene tingacite kuti titumikile Yehova mokwanila . “ Nanunso khalani oleza mtima . ” — YAK . ( Aroma 4 : 19 , 20 ) Ifenso tifunika cikhulupililo colimba . ( 2 Maf . 4 : 1 - 7 ) Komanso , ndi thandizo la Yehova , Yesu mozizwitsa anapeleka cakudya , ngakhale ndalama pamene kunakhala kofunikila . — Mat . Iye anati : “ N’nali kupemphela kwa Yehova nthawi zonse kuti anithandize . ” ( Mat . 24 : 51 ) Monga atumiki a Yehova , sitifuna kuonetsa cikondi caciphamaso . Ngati nthawi zonse tikumbukila mfundo imeneyi , tidzawathandiza bwino ophunzila athu . Mwacitsanzo , Mfumukazi yoipa Yezebeli , inalamula kuti Naboti aphedwe kotelo kuti Ahabu mwamuna wake atenge munda wa mpesa wa Naboti . Ndiponso akulu mumpingo angakuthandizeni cifukwa cakuti ndi okhwima mwa kuuzimu . ( Ŵelengani Yakobo 1 : 19 . ) Lemba la Yoswa 6 : 10 - 15 , 20 limakamba kuti asilikali a Isiraeli anazungulila mzinda wa Yeriko kamodzi pa tsiku kwa masiku 6 . N’nakhala kalembela wa gulu limenelo , ndipo umenewu unali udindo wapamwamba . N’nayankha kuti : “ Sin’nawasiyile dala . Kodi anapatsidwapo uphungu wokhudza mmene amacitila zinthu kwa wina na mnzake ? Ndiye cifukwa cake tifunika kukhala maso mpaka pamene cisautso cidzayamba . “ Inu Ndinu Mboni Zanga , ” 7 / 15 ZIMENE BAIBULO IKAMBA : Atumiki ena a Sauli anamva kuti Davide anali woimba waluso ndiponso mwamuna wankhondo . Nidziŵa mmene cimvekela ngati ufuna kucita cinthu koma sukwanitsa kucicita cifukwa colemala . Yehova adzagwilitsila nchito Ufumu kugwilizanitsa banja lake la kumwamba ndi la padziko lapansi . Nkhani yoyamba idzafotokoza zimene tingacite ngati tamva mfundo za dziko zimene zingamveke zokopa . Khalani na umoyo wosalila zambili ndi wa dongosolo . — Luka 12 : 15 N’cifukwa cake amene akuyesa kuti ali cilili asamale kuti asagwe . ” Mumaiona bwanji nkhani ya ufulu wocita zinthu ? 8 : 26 - 31 ) Filipo anacitapo kanthu mwa kuthandiza ndunayo kudziŵa coonadi molondola . Kodi nowa anangokhala zii kapena anali kuwauza kuti ‘ aliyense adziŵe zake ? ’ Kumbukilani kuti nayenso mtumwi Petulo anacita mantha ndi kuyamba kukaikila . ( Onani pikica kuciyambi . ) ( b ) N’cifukwa ciani wopha munthu mwangozi anali kufunika kukaonana na akulu ? Kwa zaka zambili , anthu oculuka aŵelengapo buku la Danieli , koma sanalimvetsetse . Inde , popeza kuti Yehova analenga zinthu zonse , iye ali na ufulu wonse wolamulila anthu kuphatikizapo zolengedwa zauzimu . 10 : 7 ) Conco , pa usiku womaliza uja , iye anawalimbikitsa kuti ayenela kupilila pa nchito imene anawapatsa . ( Mat . mu Utumiki Wathu wa Ufumu wa August 2011 . Anthu anavala bwino , anali ndi nkhope zacimwemwe , ndipo anandilandila ndi manja aŵili . Koma mtumwi Paulo anawalimbikitsa kuti “ akhale amaganizo amodzi mwa Ambuye . ” ( Afil . Iwo amakhulupilila kuti Mulungu amaona anthu kuti ndi acabecabe . Kodi kukhala na umoyo wosalila zambili kumatithandiza bwanji kutumikila Mulungu momasuka ? M’mbili yonse ya anthu , tsunami ameneyu ndi amene anapha anthu ambili . 23 : 14 - 16 ) Kodi munthu wina akanakwanitsa bwanji kulosela zinthu zimenezi popanda kuthandizidwa ndi munthu wamphamvu kuposa ena onse ? 11 , 12 . ( a ) Kodi Yehova amathandiza bwanji atumiki ake ? Conco kuti phunzilo likhale lopindulitsa , anali kukonzekela mwakhama . Yosefe anauza wopelekela cikho kuti Farao adzam’tulutsa ndi kumubwezela pa nchito yake yakale . Tingapewe bwanji kuseŵenzetsa molakwa ufulu umene Mulungu anatipatsa ? N’cifukwa cake ndife ogwilizana . 6 : 1 - 4 ; Yuda 6 ; Chiv . 12 : 3 , 4 ) Pamene angelowo anacoka m’banja la Mulungu , anayamba kulamulidwa na Satana . 4 : 1 - 9 ) Masiku ano , Satana wakwanitsa kusoceletsa anthu ambili , ndipo wawacititsa kuti adzionetsa mtima wodzikonda m’njila zosiyana - siyana . ( Aroma 5 : 12 ) Munthu woyamba , Adamu , anacimwila dala mwa kusamvela Mulungu . Ndiponso , ciukililo ca Yesu cinapeleka ciyembekezo kwa otsatila ake kuti naonso adzaukitsidwa . Munda umenewo unali wokongola komanso malo abwino okhalamo . Ngakhale kuti mwakalamila kwa nthawi yaitali , pali zambili zimene mungacite kuti mulimbitse ubale wanu ndi Mulungu . ( a ) N’cifukwa ciani anthu okonda zinthu zakuthupi amalephela kuona cuma moyenelela ? Ngakhale ndi conco , munthu amene safuna kugwila nchito yambili amakhala ngati kapolo cifukwa cakuti amacita zinthu mokakamizika . Koma kodi Mulungu amakwanilitsa bwanji malonjezo ake ? N’zoona kuti sitinapatsidwe udindo wotsogolela mtundu wa anthu monga umene Yoswa anapatsidwa . Iye anali mnyamata wooneka bwino , ndipo ayenela kuti anali ndi zaka zapakati pa 13 ndi 19 . ( Onani mapalagilafu 11 - 13 ) ) Makolo amene amapeleka citsanzo cabwino , amacita zimene amaphunzitsa . 4 : 6 , 7 , 13 ) Muzipewa zinthu zimene zingacititse kuti mucite ciwelewele . Kunali kukwanilitsa lonjezo limene Yehova anapeleka kale - kale kwa bwenzi lake Abulahamu . Makope oposa 230 miliyoni a buku limeneli asindikizidwa m’zinenelo zoposa 260 . Koyamba , Yesu atangobatizika mu mtsinje wa Yorodano , Yehova anati : “ Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa , amene ndimakondwela naye . ” ( Mat . Kodi wamasalimo anali kukhulupilila ciani cimene cinamulimbikitsa ? Akanalandila cilango ca Mulungu , sembe sanakumane na mavuto amenewo . Muyenela kudziŵa pasadakhale zinthu zimene muyenela kupewa kuti cisumbali canu cikhalebe coyela . 5 : 31 ) Pempho limeneli lidzayankhidwa pamene Yehova adzawononga dziko loipali la Satana . Tsunami amene anacitika mu 2004 atatha , boma linaika njila zocenjezela anthu m’madela onse okhudzidwa kuti ateteze miyoyo ya anthu ku ngozi yofanana . 10 : 24 ) Conco , tiyenela kumaganizila kwambili za umoyo wa abale na alongo athu kuti tiwalimbikitse pamene kuli kofunikila . Kodi Yesu anali kusankha bwanji mabwenzi ake ? Tangoganizilani mmene umoyo udzakhalila pamene aliyense “ woona Mwana ndi kukhulupilila ” adzakhala ndi moyo wamuyaya . M’nkhani yathu yotsatila , tidzaphunzila za fanizo lina la Yesu lokhudza anamwali 10 . ( Mat . Fodya ali ndi mankhwala ochedwa nikotini amene amasokoneza ubongo kwambili . Onsewa ndi mabodza a Satana . ( Luka 22 : 42 , 43 ) Mofananamo , Mulungu angagwilitsile nchito mnzathu kutiuza mau olimbikitsa a panthawi yake . 2 : 3 , 4 ) Onse aŵili ayenela kuzindikila mmene mnzake akumvelela ndiponso pankhani yokhudza mangawa a mucikwati . — Ŵelengani 1 Akorinto 7 : 3 , 4 . Pofotokoza ziphunzitso za Origen , Ambrose , ndi Jerome , buku lina linati : “ Iwo anali kufufuza zocitika zilizonse za m’Malemba ndi zimene zinali kuimila ngakhale kuti zinali zosafunika kwenikweni . 19 : 5 , 6 ; Aheb . Omasulila Baibulowo anaona kuti kugwilitsila nchito dzina la Mulungu “ sikunali kofunika ngakhale pang’ono . ” Mau amenewa aonetsa kuti mufunika kuganizila zimene mungacite kuti mulimbitse ubwenzi wanu na Yehova , na kukhalabe okhulupilika kwa iye mosasamala kanthu za mavuto amene mungakumane nawo . 1 : 1 - 3 . Pamisonkhano , timaphunzila zinthu mwa kumvetsela mwachelu nkhani za m’Baibulo , zitsanzo , ndi mbali ya kuŵelenga Baibulo . Nimamvela monga mmene wamasalimo anamvelela pamene anati : “ Malingalilo osautsa atandiculukila mumtima mwanga , mau . . . otonthoza [ a Yehova ] anayamba kusangalatsa moyo wanga . ” Boma limenelo lidzafunika kuthetsa nkhondo cifukwa ndilo vuto lalikulu limene limacititsa umphawi . CAKA COBADWA : 1987 16 : 35 ; 26 : 10 ) Ndipo panthawi imodzimodziyo , Yehova anapulumutsa Aroni , kuonetsa kuti iye anali wansembe weniweni ndipo anali kulambiladi Mulungu . — Ŵelengani 1 Akorinto 8 : 3 . 10 : 7 . Tiyeni tione mmene tingaonetsele mwa zocita zathu kuti timakhulupilila kuti “ Yehova Mulungu wathu ndi Yehova mmodzi . ” Mose anapita ku Iguputo kukapeleka uthenga wa Mulungu kwa Farao , ndipo zimenezo zinam’kwiitsa Farao . 17 : 3 . 2 , 3 . ( a ) Ndi ngozi yotani imene tingakumane nayo ngati sitiyamikila pa zinthu zabwino zimene tili nazo ? Mwacitsanzo , mukaona cinthu codabwitsa cimene Yehova analenga , dzifunseni kuti , ‘ Kodi cimeneci cikundiphunzitsa ciani ponena za Yehova ? ’ Aikapo Mateyu 6 : 9 , 10 ndi Danieli 2 : 44 . Mosiyana na Mulungu wacilungamo ndi wacifundo , Afarisi anali kuweluza anzawo kuti ni ocimwa ndi kuti sangasinthe . Kuti mudziŵe zambili , onani Zakumapeto 1 ndi 2 mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika . Baibulo imeneyi ipezekanso pa Webusaiti ya www.jw.org . Ngakhale kuti tikukhala ku dela kumene mayendedwe ndi ovuta , ndipo timafunika kuyenda mitunda yaitali , timacita zonse zothekela kupita kukalalikila kulikonse kumene tingapeze anthu . — Mat . 13 , 14 . ( a ) Ndi pa zocitika monga ziti pamene Yehova ‘ angatisiye kuti atiyese ’ ? Mulungu anati : “ Uike Yoswa kukhala mtsogoleli ndipo umulimbikitse ndi kumulimbitsa , cifukwa ndiye adzawolotsa anthuwa ndi kuwacititsa kulandila dziko limene ulionelo kukhala colowa cawo . ” ( Deut . Tidzakambilananso mafunso awa : Kodi kupeputsa malamulo a Mulungu tiyenela kukuona motani ? M’malomwake , amakhala na ciyembekezo ceni - ceni ca m’tsogolo ndipo izi zimawalimbikitsa ‘ kufunafuna mtendele ndi kuusunga . ’ — Sal . Atate anali acikulile kale pamene n’nabadwa . Tiyeni tikhale osamala kwambili kuti tisakhumudwitse ena . — Ŵelengani Aroma 14 : 5 , 13 , 15 , 19 , 20 . 32 Kodi Mtengo Ukadulidwa Ungaphukenso ? 22 : 3 ) * Marilyn atangopita anayamba kusoŵa banja lake , ndipo nayenso mwamuna ndi mwana wake anayamba kumusoŵa . ( Sal . 34 : 14 ) Mtumwi Paulo mosapita m’mbali anaonetsa mfundo imeneyi pamene analemba kuti : “ Aliyense wochula dzina la Yehova aleke kucita zosalungama . ” Ndiyeno nkhondoyo ili mkati , anatumizidwa ku msasa wina ku Ravensbrück pafupi ndi mzinda wa Berlin . Nthawi zokwanila 7 zinayamba zaka zambilimbili Yesu asanabwele pa dziko lapansi , ndipo zinapitiliza ngakhale atabwelela kumwamba . Mtumwi Paulo anafotokoza kuti : “ Malipilo a ucimo ndi imfa , koma mphatso imene Mulungu amapeleka ndi moyo wosatha kudzela mwa Khristu Yesu Ambuye wathu . ” Kukulitsa cidwi . Tingacite zimenezi mwa kukhala odzicepetsa ndi kuzindikila kuti pali zinthu zina zimene sitidziŵa , ndiponso kukhala wokonzeka kukhululukila ena ndi mtima wonse . Kodi Yehova ndi bwenzi lathu lapamtima m’njila yotani ? Popeza kuti Yehova ndiye anayamba kutikonda , watiphunzitsa mmene tingaonetsele kuti timam’konda . Nditabatizidwa , ndinatumikila ku Rhode Island kwa zaka 16 , ndipo kumeneko ndinapeza mabwenzi ambili . Nili mwana , n’nali kukonda kucita maseŵela amenewa . Anthu ena a m’nthawi ya Paulo anamunena kuti anali “ wobwetuka ” wosadziŵa zinthu . Koma tifunika kukambilana mafunso aya : Tingaonetse bwanji kuti timayamikila ufulu umene tili nawo ? NYIMBO : 41 , 89 Ngati timaika cifunilo ca Mulungu patsogolo m’malo mwa zofuna zathu zadyela , tidzatengela cikhulupililo ca Sara . ( Ŵelengani Yuda 9 . ) Pofuna kudzipenda ngati timaona ndalama moyenela , tingacite bwino kuyankha mafunso awa moona mtima : ‘ Kodi nimakhulupililadi malangizo a m’Baibo pa nkhani ya ndalama ? Mwacitsanzo , mogwilizana ndi Baibulo lacingelezi , lemba la Yobu 10 : 1 linali ndi mau 27 m’Baibulo lakale , koma tsopano lili ndi mau 19 okha . ( Aheberi 4 : 12 ) Kudziŵa zimene Baibulo limaphunzitsa ndi kuyesetsa kucita zimene limakamba , kwathandiza anthu ambili kusiya cinyengo ndi kuyamba kucita cilungamo . Anafunika kusiya umoyo wawo wabwino ndi kukakhala umoyo wosamuka - samuka . Baibo imati : “ Palibe ngakhale mmodzi wa iwo amene angathe kuwombola m’bale wake , kapena kumupelekela dipo kwa Mulungu . . . N’ciani cimene alambila onse a Yehova ayenela kucita ? Mwamsanga , Yesu anatambasula dzanja lake ndi kum’gwila ndipo anati : “ Wacikhulupililo cocepa iwe , n’cifukwa ciani wakaikila ? ” — Mateyu 14 : 24 - 32 . Tingalimbane bwanji ndi Satana kuti tipambane ? Kuti musatenge mbali m’zandale , pewani kuonelela kapena kuŵelenga zinthu zimene zimakometsa mbali imodzi pandale . Zimene timacita ngati ena atikhumudwitsa zingakhudze ulaliki wathu ( Onani palagilafu 14 ) Ndiponso , Baibulo limati : “ Ciliconse cimene tingamupemphe mogwilizana ndi cifunilo cake , amatimvela . ” Mofananamo , mwana pang’onopang’ono angataike mwa kuuzimu ndi kuloŵela njila yoipa . Iye angasoceletsedwe ndi mabwenzi oipa kapena zosangulutsa zosayenela . ( Miy . Cikondi cidzatithandize kucita zinthu zoyenela kwa anzathu . 9 Tengelani Citsanzo ca Mabwenzi Apamtima a Yehova Ana anu ndiwo maphunzilo anu a Baibo ofunika kwambili , ndipo afunika ‘ kuphunzila ndi kudziwa ’ za Yehova kuti akapeze moyo wosatha . Koma poyamba , tonse atatu anatiika ku mpingo wina m’tauni ya Quezon , mmene anthu ambili anali kukamba Cizungu . Mofanana ndi zimene zinaloseledwa , Yosiya anatumiza anthu kuti “ akatenge mafupa m’mandawo , ndipo anawatentha paguwa lansembelo ” ku Beteli ( 2 Mafumu . Conco Yehova anamuuza kuti : “ Iwe ukufuna - funabe zinthu zazikulu . N’zocitika ziti zimene zingapangitse makolo kubwelela ku mpingo wa cinenelo cimene ana awo amamvetsetsa ? Kwa ine , izi zinali zosamveka . Kapena kodi nyumba yanu ya Ufumu ikukonzedwanso ? 18 “ Mau a Mulungu Wathu Adzakhala Mpaka Kalekale ” Nimaona kuti ni mwayi waukulu kuti Yehova wanilola kugwila nawo nchito yake . Koma kodi iye angalephele kukwanilitsa Mau ake ngati sinicita zambili pom’tumikila ? ’ Mamiliyoni a tumabuku tumenetu anatugaŵila kwaulele . Kodi Aisiraeli anali kuweluza bwanji mlandu wa kupha munthu mwadala ? 1 : 26 ) Iwo anali kudzakhala ana ake , ndipo Yehova anali kudzakhala Atate wawo . Ophunzila a Yesu amene anali m’cipinda capamwamba sanaiŵale zimene zinacitika patsikulo . Ndinasangalala kwambili tsiku lina pamene amuna anga anandiuza kuti afuna tipitile pamodzi kumisonkhano . Nanga Yohane anali wotani ? Kodi mwaziona zinthu zitatu zimene Mulungu afuna kuti tikhale nazo ? Dzinali limatikumbutsa kuti Satana anaipitsa dzina la Yehova mwa kunena kuti iye ndi wabodza . M’Baibo muli nkhani zambili zosonyeza mmene Yehova anaonetsela cifundo kwa anthu . Mu October 1958 , Ilse ndi Elfriede anayamba kuphunzila nane Baibulo . Ndinabatizika patapita miyezi itatu mu January , 1959 . Adani amenewa akanakwanitsa kuononga Mabaibulo onse , sembe kulibe Baibulo masiku ano . ( b ) Kodi wacicepele wina anaseŵenzetsa bwanji mpata wolalikila umene anapeza kusukulu ? Sarie ananenanso kuti : “ Palibe nchito ina imene imandikondweletsa kuposa yolalikila . Ndipo mwa mzimu wake woyela , Yehova amatipatsa mphamvu yotithandiza kupitiliza kugwila nchito yopulumutsa moyo imeneyi . ” Yesu anati : “ Wonyenga iwe ! Koma iwo amaiŵala kuti olo kuti anthufe tili na ufulu wosankha zocita , sitinalengedwe na udindo wodziikila tekha miyezo ya cabwino na coipa . Tinali kuuza atsikana athu kuyelekezela kuti ni Mboni imene ikuyankha mafunso . Masiku anonso miyoyo ya anthu ili pangozi . 1 : 18 ; 1 Yoh . 2 : 15 - 17 ) Maganizo a anthu onyalanyaza colinga ca Yehova amenewa ndi maloto cabe . Pamene ticita zimenezi , tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi izi zindiphunzitsa ciani ponena za Yehova ? Ubatizo wanu ni cizindikilo cakuti munadzipeleka kwa Mulungu . Iye anatsatila citsogozo ca Mulungu , anacita cifunilo ca Yehova , ndipo anatsatila njila yabwino ya moyo . — Yoh . N’zolimbikitsa ngako kudziŵa kuti Yehova amamvetsetsa mmene timvelela , ndipo amatipatsa citonthozo cofunikila . Buku linanso limakamba kuti madela ena ku Isiraeli kulibiletu mitengo masiku ano . Pa kacisi , anali kulambila ndi kutamanda Yehova mogwilizana . Anthu a Yehova akusangalala ndi paladaiso wauzimu amene ali m’mbali ya padziko lapansi ya gulu la Mulungu . Mau akuti “ okonda zosangalatsa ” amakamba za anthu ‘ otengeka ndi . . . zosangalatsa za moyo uno . ’ — Luka 8 : 14 . ( Eks . 14 : 21 , 22 , 29 , 30 ) Iwo anacita zinthu mogwilizana , ndipo “ khamu la anthu a mitundu yosiyanasiyana ” amene sanali Aisiraeli anapita nao limodzi . Iye anasangalala ndi akuluwo cifukwa anali abusa odzipeleka ndipo ena mwa io anali acikulile ngati atate ake . Funso limeneli n’locititsa cidwi cifukwa Yesu anati : “ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” Ngakhale n’conco , iwo anali kukanganabe zakuti n’ndani anali wamkulu pakati pawo . Tingatengele citsanzo cake mwa kulemekeza zimene ena amakhulupilila . Pamenepo matenda ake anathelatu ! Ufumu wa Mulungu udzapindulitsa makamaka anthu onse amene amaupemphelela ndi mtima wonse komanso amene amacita zinthu mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu . Pamene Mulungu analenga dziko lapansi , angelo ‘ anafuula pamodzi mokondwela , ndipo ana onse a Mulungu anayamba kufuula ndi cisangalalo . ’ César anakamba kuti : “ Kwa nthawi yoyamba , n’nadziŵa colinga ca moyo . ( Eks . 35 : 5 ; 1 Mbiri 29 : 5 - 9 ) M’nthawi ya Mfumu Yehoasi , ansembe anakonza zinthu zowonongeka pa nyumba ya Yehova poseŵenzetsa ndalama zimene anthu anapeleka . Muloleni kuti akuphunzitseni kulela bwino ana anu . Muziseŵenzetsa malangizo amene iye amapeleka kupitila m’Mau ake na gulu lake . Koma izi sizitanthauza kuti Mulungu ali kutali ndi ife . Kodi kukhala wolimba mtima kumatanthauza ciani ? Koma kuti nyumba ikhalebe yolimba , khama n’lofunika . Iwo ‘ akupitiliza kupeza mphamvu kucokela kwa Ambuye . ’ Anadziŵanso kuti pakapita zaka zambili , iwo adzakhala “ m’masiku otsiliza , ” amene ni “ nthawi yapadela komanso yovuta . ” ( 2 Tim . Kupyolela m’pangano la mu Edeni , Yehova anapeleka ciweluzo kwa njoka ndi mbeu yake . Njoka ndi mbeu yake zikuimila Satana Mdyelekezi ndi onse amene ali kumbali yake potsutsa ulamulilo wa Mulungu . M’kupita kwa nthawi , n’nazindikila mfundo ina yofunika yakuti , nthawi zonse pamakhala abale ofikapo amene angakuthandize malinga ngati uwalola kutelo . Kutanthauza kuti inali nchito yovuta kwambili . ( Yesaya 6 : 8 ) Akristu ambili , monga amene analowa Sukulu ya Giliyadi , anasamukila kumaiko akutali . 119 : 11 . ( Yobu 2 : 7 ) Mavuto ake anawonjezeka cifukwa ca mau opweteka ndi ofooketsa a mkazi wake ndi a anzake atatu acinyengo . — Yobu 2 : 9 ; 3 : 11 ; 16 : 2 . NYIMBO : 8 , 54 Nkhani iliyonse pa mbali imeneyi inakonzedwa kuti ikuthandizeni kulimbitsa cikhulupililo canu pa mfundo inayake ya m’Baibulo . 3 : 12 ; 1 Pet . Sara anakamba kuti : “ Panapita zaka zitatu nikukhala movutika , koma cifukwa ca thandizo la Yehova , n’nakwanitsa kupilila . ” Tikamasinkhasinkha ndi kuyamikila zinthu zabwino zimene Yehova waticitila , tidzakhala ndi mzimu woyamikila . Ndiponso kusiyana maganizo ndi wina wake mumpingo ndi cinthu covuta kwambili kupilila . LIU lakuti “ Eureka , ” limatanthauza “ Ndacipeza ! ” Wasayansi winanso anakamba kuti “ mphamvu imene [ dzuŵa ] limatulutsa . . . pa sekondi imodzi cabe ni yokwanila kuthandiza anthu pa moyo wawo kwa zaka 200,000 ! ” Mkazi wake anati : “ Kuŵelenga nkhani za m’mabuku athu monga nkhani zakuti , ‘ Kodi Mungakatumikile Kudziko Lina ? ’ Koma pa nthawiyi , anali kutumikila monga mpainiya wapadela mu mzinda wa Dumaguete , ndipo n’napita kukam’cezela . Tikaganizila Malemba onsewa okamba za kuukilidwa komaliza kwa anthu a Mulungu , timatha kuona kuti Gogi wa Magogi si Satana , koma ndi mgwilizano wa mitundu . Pa sukuluyi m’pamene ndinadziŵila Gwen , ndipo tinayamba kuvinila limodzi . ( Ŵelengani Yohane 14 : 27 . ) Cifukwa ca mmene anali kuzipangila , nsapatozo zinali kukhala zolimba ndi zosavuta kuyenda nazo . Ganizilani mmene Adamu anaseŵenzetsela ufulu wake m’njila yoyenela . Olosela zakutsogolo amaona mmene anthu ofunsilawo acitila zinthu na mmene ayankhila powafunsa mafunso . Pa anthu onse amene anakhalapo padziko lapansi , Yesu Kristu ndiye munthu wofunika kwambili kumutsatila . Koma kumbukilani mau olimbikitsa amene Yehova anauza Yoswa . 2 : 22 ) Timoteyo sanali waulesi . Maganizo otele angacititse munthu kukhala wosasangalala . Kupatsa kumapindulitsa inu ndi ena Ena amaopa kukhala osiyana ndi anzawo kunchito kapena kusukulu . Atumiki a Mulungu amayesetsa kuthandiza anthu ena . Mfundo imeneyi ingatithandize pa mafunso ambili amene tingakhale nawo mu umoyo , monga akuti : ‘ Kodi cimene nifuna kucita cili m’gulu la nchito za thupi ? ( b ) Kodi mau a Davide a mu Salimo 61 , amakukumbutsani bwanji citsanzo cabwino ca Hana ? Ndi motani mmene Mulungu amaonela atate anga amene ndi Msilamu ? ( 2 Mafumu 20 : 1 - 6 ) Koma Davide sanayembekezele kuti Mulungu amucilitsa mozizwitsa . Iwo anati : “ Timakondwela kwambili kudziŵa kuti tikugwila nao nchito imene idzapindulitsa gulu la padziko lonse . ” 18 , 19 . ( a ) Kodi abale na alongo ofikapo kuuzimu angathandize bwanji acicepele ? Koma kodi inu muli na cikhulupililo monga cimene Marita anali naco cakuti m’tsogolo okondedwa anu amene anamwalila adzauka ? Pamene tikuyembekezela kukwanilitsidwa kwa “ nkhani yosangalatsa ” imeneyi yokhudza Mfumu Mesiya , tiyeni tisaleke kudziŵikitsa dzina lake . M’fanizo lake la Msamariya , Yesu anatithandiza kudziŵa tanthauzo la kuonetsa cikondi ndi cifundo . Iye anali kukhulupilila kuti Yehova adzamusamalila ndi kum’teteza . ( 1 Akor . 15 : 9 ) Pambuyo pake analemba kuti : “ Ine , munthu wocepa pondiyelekeza ndi wocepetsetsa wa oyela onse , ndinapatsidwa kukoma mtima kumeneku kuti ndilengeze kwa mitundu ina uthenga wabwino wonena za cuma copanda polekezela ca Khristu . ” Musamayembekezele zambili . — Mika 6 : 8 Anthu amene tawachula m’nkhani ino , Sakura , Ribeiro , Stephen , ndi Hans , anacita khama kuti aleke makhalidwe oipa . Koma n’nawafotokozela kuti n’colinga ca Mulungu kuti tizilalikila za Ufumu wake . Mwacitsanzo , bwana wa kampani ina yaikulu yazomanga - manga anaona kuti Mboni za Yehova ndi zokhulupilika . Mabaibulo oposa 5 biliyoni afalitsidwa , kaya athunthu kapena mbali yake . ( b ) Ndi malangizo otani amene Yehova amatipatsa otilimbikitsa kukhala ogwilizana ? Ndiye cifukwa cake Rakele , mkazi wa Yakobo , anadandaula ataona kuti mkulu wake akubala ana koma iye ayi . Ndi ciyeso cotani cimene cidzakhalapo pambuyo pa kuonongedwa kwa “ Babulo Wamkulu ” ? 4 : 16 , 17 ) Conco , nkhondo ya Aramagedo isanayambe , Akristu onse odzozedwa amene ndi “ mkwatibwi ” adzakhala ali kumwamba . Kukonda Mulungu ndiye kofunika kwambili ndipo kumatilimbikitsa ngako . Nchito imapita patsogolo ngati tiphunzitsa acinyamata kuti akatenge maudindo . Ŵelengani Mateyu 6 : 26 . Funsani wophunzila kuti , ‘ Ndi zolinga zotani zimene muli nazo ? ’ TSAMBA 23 • NYIMBO : 112 , 101 Pa tsikulo , anthu mamiliyoni akakumbukila imfa ya Khristu . Amene ali m’madela akumidzi asadzaloŵe mumzindawo . ” Conco , ndinapempha mkazi wanga amene ali ndi zaka 63 kuti tiphunzile cinenelo ca Cichaina . Kodi lemba la Yesaya 40 : 29 lingatilimbikitse bwanji ? Koma ngati timayesetsa kulimbana ndi zilakolako zoipa , tidzapewa ciwelewele ndi mavuto amene amatsatilapo cifukwa ca khalidweli . ( Agal . N’nakondwela kubwelelanso kumene n’nayambila utumiki wanthawi zonse wapadela zaka zoposa 40 m’mbuyomo . Tingawatsatile motani maganizo amene Kristu Yesu anali nao ? Ganizilani kuti mukuona Debora ndi Baraki akuyang’ana pamwamba pa Phili ndipo zovala zao zikuuluzika ndi mphepo yamphamvu . Atate acikristu amatsanzila Yehova mwa kuphunzitsa ana ao coonadi ndi kuwathandiza kukhala paubwenzi ndi Atate wao wakumwamba ( Onani ndime 8 - 10 ) Conco , io anaitananso anthu olemekezeka , kuphatikizapo nduna yaikulu ya boma , aphungu a nyumba ya malamulo , abusa a zipembedzo , ndi akuluakulu a asilikali . ( Ŵelengani 1 Akorinto 7 : 29 - 31 . ) Muziphunzilapo kanthu pa zimene mwalakwitsa kuti musakabwelezenso zimenezo Tikaonanso lemba la Yohane 3 : 16 , lili ndi mau akuti “ aliyense wokhulupilila [ Yesu ] asaonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” Kodi Yehova anawathandiza bwanji Aisiraeli kuona kuti moyo wa munthu ni wopatulika ? N’cifukwa Ciani Zigaŵenga Anali Kuzithyola Miyendo Pozipha ? Ndikakuona ukusintha kukhala munthu wabwino , ndimakondwela kwambili . Yakobo anati : “ Lilimenso ndi moto . ” Cifukwa cina n’cakuti , sanavomeleze ciphunzitso ca moto wa ku helo , cifukwa anaona kuti kuzunza anthu koteloko n’kupanda cilungamo ndi cikondi . 1 , 2 . ( a ) Kodi Yehova amafuna kuti anthu ake akhale ndi khalidwe lotani ? Yosefe anafotokoza kuti maloto aŵili a Farao anali ndi tanthauzo limodzi . Pankhani ya zakudya , zovala , ndi malo okhala , Yehova amadziŵa bwino - bwino kuti ‘ uyu afunika izi , uje afunikila ici . ’ N’ciani cinathandiza Yesu kukhalabe wokhulupilika pamayeselo ? Mwacionekele , pamene muphunzila Baibo ndi ana anu kapena anthu ena , mumaŵelenga Aroma 5 : 12 pokambilana za colinga ca Mulungu cokhudza dziko lapansi , dipo , na mkhalidwe wa akufa , m’nkhani 3 , 5 , na 6 . Pamene mukambilana nao nkhani zovuta monga za cibwenzi , samalani kuti simugogomeza kwambili pa kupeleka macenjezo . Koma muziphunzitsa ana anu njila yoyenela yothetsela vutolo . Yehova anauzila mneneli Danieli kulosela kuti m’nthawi yamapeto , anthu “ adzadziŵa zinthu zambili zoona . ” Ngakhale n’conco , tiyenela kuonetsetsa kuti kulambila kwathu kwa pabanja kumacitika mokhazikika . Cosankha canu cotumikila Yehova si cosankha cokha cimene cimakhudza tsogolo lanu . Anam’tumizila angelo kuti am’tumikile , anapeleka mzimu Woyela kuti um’thandize , ndipo anam’tsogolela posankha atumwi 12 . Kodi kuganizila madalitso amene tili nao kumatithandiza bwanji kulimbana ndi mavuto ? Magazini ino ya Nsanja ya Mlonda , ifotokoza mmene Mulungu amatitonthozela . Masiku ano , n’zosatheka kupewelatu “ zinthu zosayembekezeleka ” kapena kupewa kupezeka pamalo olakwika komanso panthawi yolakwika . Koma kudzicepetsa n’kofunika kuti mukhale pansi pa “ dzanja lamphamvu la Mulungu , ” ndi kuti ‘ mumutulile nkhawa zanu zonse . ’ ( 1 Pet . Koma atapeza mipukutu ina , zenizeni zinadziŵika . 102 : 12 , 27 ) Iye anapeza citonthozo podziŵa kuti nthawi zonse Yehova adzacilikiza anthu ake pamene akumana ndi mavuto . Utumiki Wanu Uli Ngati Mame ? Kodi tingathandize bwanji anthu ena kupanga zosankha zaumwini ? Yehova amapeleka citonthozo ca panthawi yake kupitila mwa Yesu Khristu , Malemba , ndi mpingo wacikhristu . Mwa kupatsa mwana wathu kapena wophunzila Baibo cilango ca m’Malemba , tingamuthandize kukwanilitsa colinga cokhala wotsatila wa Khristu . 6 , 7 . ( a ) Kodi Baibo imaseŵenzetsa liu lakuti “ thupi ” m’njila zina ziti ? ( Aroma 2 : 28 ; 1 Akor . Kodi mudzayesetsa kukhala olimba mtima m’mbali zonse za umoyo wanu ? N’nacita mantha , poganiza kuti afuna kunicotsa nchito . N’nabadwa pa 24 April , 1931 , ndipo ndine mwana waciŵili pa ana awo anayi . 8 , 9 . ( a ) Kodi pa msonkhano wa mkati mwa wiki timalandila malangizo ati othandiza ? 8 - 10 . Mukatelo , mudzamuyandikila kwambili Atate wanu wakumwamba . N’citsanzo citi ca m’Cilamulo ca Mose coonetsa mmene Yehova amaonela anthu ake ? Kaŵilikaŵili , abusa amene amapatsidwa ndalama amalalikila kwa mamembala ao . ( b ) Kodi Yesaya 46 : 10 , 11 ndi 55 : 11 limatitsimikizila ciani ? Nthawi ina , Yehova anapempha mneneli Yesaya kuti akhale wom’lankhulila wake . Koma panthawiyo Hiberi sanali panyumba . Kodi Khristu akanacita bwanji pamenepa ? Ticite zimenezi podziŵa kuti Yehova adzatipatsa mphoto pa nthawi yake . — Ŵelengani Akolose 3 : 23 , 24 . Mwacitsanzo , ganizilani za m’bale wina wa pabanja amene anaona kuti cangu cake pa nchito yolalikila cayamba kucepa . Mu 1961 , makalata ocokela ku ofesi ya nthambi olimbikitsa kuyamba upainiya anaŵelengedwa m’mipingo . Kumiko atayang’ana kumbuyo zaka monga 10 za utumiki wake Nepal , anati : “ Mavuto onidetsa nkhawa anagaŵikana ngati Nyanja Yofiila . Mbeu zimaimila uthenga wa Ufumu umene umalalikidwa kwa a mtima wofuna coonadi . Mwina muganiza kuti cosankha cimeneci cinali cosavuta cifukwa nthawi zonse kutumikila Yehova ndiye cinthu canzelu ndi copindulitsa . ( Luka 22 : 36 , 38 ) Ise Akhristu tifunika kusula malupanga athu kuti akhale zida zolimila . Popeza tadziŵa ena mwa anthu amene anaukitsidwa , kodi lomba tidzakambilana mafunso ati ? ( Chivumbulutso 6 : 4 ) Kuyambila mu 1914 , anthu akhala akuvutika kwambili ndi nkhondo . Kodi simukuvomeleza kuti miyezo yolungama ya Yehova ndi yabwino ndipo imatiteteza ? Kodi Akhristu afunika kusamala na ciani ? 18 , 19 . ( a ) Tingawathandize motani anthu amene akhala ofooka kwa kanthawi ? N’nali kucita cidwi ndi khama lawo panchito yofalitsa uthenga wabwino wokamba za Ufumu wa Mulungu padziko lonse . Nanga kodi Yehova akanathandiza bwanji munthu wabwinoyo ? Kodi n’zothekadi kuyandikila Yehova ? Mulungu walonjeza kuti adzapeleka “ mzimu woyela kwa amene akum’pempha . ” Awo amene ali na cikhulupililo ndipo amayamikila na mtima wonse coonadi ca m’Baibo cimene aphunzila , sawayawaya kudzipeleka na kubatizika . Timasangalala ndi nchito ya m’dela M’kupita kwa nthawi , mzimu woyela wa Yehova unalimbitsa amuna ena amene anasankhidwa kutsogolela anthu ake . Molingana na Yesu , afunika kuona kuti kucita cifunilo ca Yehova ndiye kofunika ngako mu umoyo wake . Komanso , mosakayikila mungamuuze za ciyembekezo canu ca dziko la paladaiso , limene anthu a Mulungu adzakhalamo kosatha . Mwacionekele mufuna . ( Aroma 13 : 1 - 4 ) Ngakhale n’conco , timadziŵa kuti sitifunika kuloŵelela m’zandale mwa kukondela cipani kapena wolamulila winawake . ( Yoh . ( 2 Tim . 2 : 15 ) Conco , m’nkhani ino tidzakambilana zimene tingacite kuti tilole mphamvu ya Mau a Mulungu kugwila nchito ( 1 ) mu umoyo wathu , ( 2 ) mu ulaliki , ndi ( 3 ) pophunzitsa papulatifomu . Kaamba ka zimenezi , amayamba kukangana cifukwa ca kusiyana zibadwa ndi makulidwe , ndalama , azipongozi , azilamu , ndi kulela ana . “ Odala ndi anthu amene ali ofatsa , cifukwa adzalandila dziko lapansi . ” — Mat . Komanso tonse tiyenela kucilikiza ndi kukonda kwambili abale a munthu wocotsedwayo kuti asamaone ngati akusalidwa ndi abale anzao . — Aroma 12 : 13 , 15 . ( Mat . 24 : 6 ) Aroma anaononga Yerusalemu mu 70 C.E . , ndipo anamenyanso nkhondo zing’onozing’ono ndi maufumu amene anali oyandikana nao . NYIMBO : 32 , 154 Iye anabatizika , ndipo pali pano ni mkulu mumpingowo . Cinanso cimene cingatiike pa ciyeso pa nkhani ya kudzicepetsa ni popanga zosankha . Lomba nimaona kuti nili na ufulu wopemphela kwa Yehova popanda cododometsa ciliconse . ” Koma panthawiyo , Solomo anali “ wamng’ono komanso wosakhwima . ” Njila yabwino kwambili yopewela ciwelewele ni mwa kusamala na zimene timaona . Mwamsanga Aroma analoŵa mu mzinda na kuyamba kuononga mpanda wakunja wa kacisi . Mulungu amadziŵa zosoŵa zathu . Conco , tiyeni tikambilane mafunso aya : N’cifukwa ciani cilimbikitso n’cofunika ? ( Luka 21 : 24 ) Odzozedwa sanali kudziŵa kuti ulosi wa m’Baibo udzakwanilitsidwa bwanji kweni - kweni . Pamene Davide anali wacicepele , anapha zilombo zoopsa zimene zinagwila nkhosa za atate wake . Ena amayamba kuganiza na kucita zinthu mwaucikulile ali aang’ono , ndipo angakhale na colinga cobatizika . 14 : 14 ) Izi zitanthauza kuti tingapemphe “ ciliconse ” cogwilizana ndi zofuna za Yehova . 3 : 15 ) Mukatelo , mungakhale otsimikiza kuti mudzapulumuka pamene dziko loipali likuwonongedwa , ndipo mudzakhala ndi moyo wacimwemwe mpaka muyaya . Kulamulilidwa ndi Mulungu kudzakhala kosangalatsa cifukwa kudzasiyana ndi maulamulilo a anthu osonkhezeledwa ndi Satana . 13 : 17 . ( Aroma 8 : 26 , 27 ; Aefeso 3 : 20 ) Tikadziŵa kuti Mulungu waloŵelelapo kutithandiza , ngakhale m’zinthu zazing’ono , ubwenzi wathu ndi iye ungalimbe . N’ciani cionetsa kuti Yesu amakonda kwambili anthu ? Ndikuona kuti ndinasankha mwanzelu . ” Ndipo tizimuonetsa kuti timam’konda ndi mtima wathu wonse , moyo wathu wonse , maganizo athu onse ndi mphamvu zathu zonse . — Maliko 12 : 30 . Cosankha cina cacikulu , cimenenso cingatibweletsele madalitso , ndi cokhudza kuyamba utumiki wanthawi zonse . Muzitumikila Yehova Mulungu wanu . ” Nthawi zambili , timakambilana mmene malonjezo a m’Baibulo akhala akukwanilitsidwila . Ndithudi , iye analidi wodzicepetsa . Sitiyenela kudabwa tikaona kuti dziko likudana nafe cifukwa ca zimene timakhulupilila popeza kuti Yesu anaticenjezelatu za zimenezi . Koma Yesu ananena kuti ndi Mulungu yekha amene adzagonjetsa imfa . [ Mau apansi ] ( Aroma 6 : 19 , 20 ) Ndiyeno tinaphunzila coonadi ca m’Baibo , tinasintha umoyo wathu , tinadzipeleka kwa Mulungu , na kubatizika . Abale anakondwela ngako na zotulukapo zabwino zimenezi ! Kodi timaceleza alendo ocokela ku maiko ena ? M’nkhani ino , tiphunzila mmene omasulila Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso la 2013 anagwilitsila nchito mfundozi . Tiphunzilanso mmene omasulila Baibuloli m’zinenelo zina amatsatilila mfundo zimenezi . Komanso , sanadziŵe kuti posapita nthawi adzakumana na vuto lalikulu lofuna nzelu kuti alithetse . Ndithudi , maphunzilo a kuuzimu ndi kukhulupilila Yehova , zinam’thandiza kuika maganizo ake pa zinthu zakumwamba . M’kati mwa masiku otsiliza , “ uthenga wabwino uwu wa ufumu ” udzalalikidwa mokwanila . N’ciani cingatithandize kukhala otsimikiza kuti malonjezo amenewa adzakwanilitsidwa ? ( Sal . 55 : 1 , 22 ) Mukacita mbali yanu kuti muthetse vuto , pemphelo la mtima wonse limathandizani kucepetsa nkhawa . Mwacitsanzo , anthu osacilikiza Cikomyunizimu anali kuonedwa kuti ni nzika zosafunika kweni - kweni . Posacedwapa Yesu adzaononga anthu onse oipa padzikoli ndi kubweletsa mtendele ndi citetezo — Ŵelengani Mika 4 : 3 , 4 . Abale a ku Lusitara anavomeleza zimenezo . Colinga ca Yehova cokhudza kulambila koona “ cidzacitika . ” Farao anakhutila ndi mmene Yosefe anamasulila malotowo . 14 : 33 . Kudzipeleka ni kulonjeza kuti tidzam’tumikila Yehova zivute zitani . Yesu anapekeka citsanzo cabwino kwambili pankhaniyi . Jairo amagwilitsila nchito maso ake pouza ena zimene amakhulupilila . ( Salimo 45 : 4 ) Nchito yake yoyamba inali kucotsa Satana ndi ziwanda zake kumwamba . — Chivumbulutso 6 : 2 ; 12 : 9 . Iye analimbikitsa oweluza Baraki , ndipo anacita mbali yaikulu pothandiza Aisiraeli kuti amasuke kwa adani ao amene anali kuwapondeleza . Kungatithandizenso kukhala wodekha ndi wokhulupilika kwa Mulungu pamayeselo . Mulungu Amakuyang’anilani 4 Ngati wina m’banja lanu wacotsedwa mumpingo , mukhoza kukhala wokhulupilika kwa Yehova . Ngati zimenezo n’zosatheka pali pano , yambani kumaceza ndi ofalitsa ocokela ku maiko ena amene ali m’dziko lanu . Conco , anthu ambili amene adzaukitsidwa adzakhalanso ndi moyo padziko lapansi . — Ŵelengani Yohane 5 : 28 , 29 ; 11 : 44 . Ngati wina adyako cakudya cimeneci adzakhala ndi moyo kosatha . Komabe , kuzionanso bwino nkhani za m’Baibo kuonetsa kuti munthu sanafunikile kukhala woyamba kubadwa kuti akhale kholo la Mesiya . Tikaphunzila za dziko ndi cikhalidwe ca anthu ocokela ku maiko ena , cidzakhala copepuka kugwilizana nawo . Timadziŵa kuti akulu mumathela nthawi yoculuka posamalila maudindo ena pampingo , ndipo mumakhala ndi nthawi yocepa yocita zinthu zina . Izi ndi zimene Baibulo limakamba pa Yesaya 14 : 7 . NYIMBO : 72 , 82 Iye sanaphunzitsidwe monga msilikali , ndipo anali asanajaile kuvala zovala zankhondo maka - maka za Sauli , amene anali wamtali kwambili pakati pa Aisiraeli . Komanso , mfundo za pa jw.org zothandiza pophunzila buku lakuti , “ Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , ” zingakuthandizeni kukhutila na zimene mumakhulupilila . Koma pamene nkhondo inatha , milandu yawo yonse inacoka washauti ndipo anawamasula onse . Koma kuphunzitsa ena kumapatsa cimwemwe . — Mac . 20 : 35 . Ganizilani kusiyana pakati pa Adamu ndi Inoki . Cifukwa ngati cinacake m’thupi mwathu cimacoka tikafa na kukakhala ndi moyo kwinakwake , sembe imfa sikanakhala cilango ca ucimo , monga mmene Mulungu anakambila . ( b ) Nanga iye anacita ciani ? Iye anawalimbikitsa kukhala ogwilizana m’cikhulupililo ndi kupitiliza kuphunzila za Kristu kuti akhale ‘ anthu acikulile , ofika pa msinkhu waucikulile umene Kristu anafikapo . ’ — Aefeso 4 : 13 . 13 Kodi Mukumbukila ? Ndipo cikumbumtima cathu cingatithandize kukwanitsa zimenezo . CIKUTO : Abale aŵili alalikila uthenga wa m’Baibulo kwa msozi ku Negombo , kumadzulo kwa doko ku Sri Lanka ▪ Yamikani Yehova Ndipo Mudzadalitsidwa Nkhani ziŵilizi , zidzatithandiza kuzindikila anthu a Mulungu , ndi kugwilizana nao potumikila Yehova . ( 2 Akorinto 5 : 14 , 15 ) Kuyamikila nsembe ya Yesu ndi mtima wonse kuyenela kutipangitsa kusintha umoyo wathu . Tisakhale ndi moyo wofuna kudzisangalatsa tokha koma tikhale ndi moyo wosangalatsa Yesu amene anatifela . 3 : 18 , 19 ; Dan . N’ciani cofunika kuti mudzipeleke ? * N’cifukwa ciani Akhristu mumpingo safunika kusankhana cifukwa cosiyana mtundu , dziko , kapena cifukwa cakuti ena ni olemela kapena osauka ? N’zoona kuti timafunikila kulalikila anthu onse . Ganizilani izi : Kucokela pamene Ufumu wa Mulungu unayamba kulamulila kumwamba m’caka ca 1914 , anthu a Mulungu anayesedwa ndipo mwa pang’onopang’ono anayeletsedwa mwakuuzimu . Mwacitsanzo Joseph wa zaka 79 , wa ku Canada anati : “ Ndimayesetsa kucita zimene ndingakwanitse m’malo moganizila kwambili zimene ndinali kucita poyamba . ” ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) Komabe , ofesi ya nthambi m’dzikolo inanena kuti “ abale a m’madela ena anayamba kutumiza thandizo m’delalo ngakhale kuti makomiti oyang’anila za cithandizo anali asanapangidwe . ” Ngakhale kuti tatumikila Yehova kwa zaka zambili , ndi bwino kuti nthawi ndi nthawi tizisinkha - sinkha za ukulu wa Mlengi wathu . ( Miyambo 13 : 4 ) Koma silitimbikitsa kugwila nchito monyanyila . Ndikufuna ndidziŵe zimenezi . ” Tikatelo , m’pamene Yehova adzatikomela mtima tikafuna thandizo . — Aef . Ngakhale masiku ano , Yehova amaganizila anthu ocokela kumaiko ena amene amasonkhana mumpingo mwathu . ( Deut . 10 : 17 - 19 ; Mal . Iye sanaigwilitsile nchito kuti aonjezele ndalama za mbuye wake , kapena kuisungitsa kwa osunga ndalama kuti apeze ciongoladzanja . OPEZEKA PA CIKUMBUTSO ( 2017 ) Iwo amacezela anthu ndi kuwaonetsa zimene Baibulo limanena zokhudza Ufumu wa Mulungu . Amayi anamwalila na zaka 86 . N’cifukwa ciani pemphelo n’lofunika kwa Mkhristu aliyense wobatizika ? Ŵelengani Aefeso 6 : 14 . Pambuyo potamba pulogalamuyo , bwanji osapatula nthawi yokambilana na banja lanu mmene mungaseŵenzetsele mfundo zimene mwamvetsela ? Sinthanani zimene mwalemba , ndiyeno yambani kuseŵenzelapo pa mbali zimenezo kuti muzionetsana ulemu . Mu 1956 pamene M’bale Nathan Knorr anaticezela , n’napatsidwa nchito yothandiza anthu pa msonkhano waukulu m’dzikolo . Funso limeneli lidzayankhidwa m’nkhani yotsatila . Kodi Malemba amakamba ciani pankhani yopumula na kusanguluka ? Pamene Yesu anali kupacikidwa , panali Jowana ndi akazi ena “ amene anali kuyenda naye limodzi ndi kumutumikila pamene anali ku Galileya . Panalinso amai ena ambili amene anabwela naye limodzi kucokela ku Yerusalemu . ” Tingathandizenso abale athu kupita patsogolo mwa kuseŵenza nao pamodzi . ( Yoh . 6 : 10 - 15 ) Tsiku lotsatila pamene anali ku tsidya lina la nyanja ya Galileya , Yesu anaona kuti maganizo ofuna kumulonga ufumu amene anthuwo anali nawo , acepako . ( Salimo 63 : 6 ) Iye anakambanso kuti : “ Ndidzatamanda Yehova amene wandipatsa malangizo . Conco , mokoma mtima iye anandiuza kuti : ‘ Yuichiro pita kunyumba ndipo ukasinkhe - sinkhe mofatsa zimene Yehova wakucitila . ’ M’dziko latsopano limene likubwelali tidzasangalala kwambili kuposa mmene timasangalalila masiku ano . Kondani gulu lonse la abale . ” — 1 Pet . ( Mateyu 6 : 33 ) Mukamataila nthawi yanu pa zosangulutsa , kodi cikumbumtima canu cimakukumbutsani mau a Yesu ? N’ciani cimene tingacite kuti tizikonda kwambili coonadi ca m’Baibo ? Koma izi zikalibe kucitika , “ Mulungu anamucitila umboni kuti akukondwela naye . ” ( 2 Akor . 4 : 7 - 9 ) Mwacitsanzo , tsiku lina pamene tinali kulalikila m’mudzi wina , anthu ena anamasula agalu awo . 21 : 17 ; Yos . Mouzilidwa na Mulungu , mtumwi Paulo analimbikitsa Akhristu anzake kuti : “ Pitilizani kuphunzitsana ndi kulangizana mwa masalimo , nyimbo zotamanda Mulungu , ndi nyimbo zauzimu zogwila mtima . Kodi Ophunzila Baibo oyambilila anatenga kaimidwe kanji kulinga ku zipembedzo zonama ? 39 : 7 ) Koma Wolamulila Wamkulu wa cilengedwe conse sadalila amtolankhani kudziŵitsa anthu za iye . Ndikawayankha tinali kukangana , cifukwa tonse tinali kuona wina kukhala wolakwa . Conco , kukambilana za makonzedwe a mizinda yothaŵilako , kudzatithandiza kudziŵa mmene Yehova amaonela ucimo , anthu ocimwa , na kulapa . Mwinanso tinali na luso la zoimbaimba kapena la zamaseŵela , limene likanaticititsa kukhala wochuka komanso wolemela m’dzikoli . Koma zonsezo tinazisiya . ( Aheb . Komanso , kumbukila kuti suyenela kuyankha munthu aliyense amene angofuna kutsutsana nawe , kapena wongofuna kuseka zimene umakhulupilila . — Miy . 3 : 5 ) Zilakolako zoipa zingakhale zamphamvu kwambili , ndipo zingasokoneza ubwenzi wathu na Yehova na kutitayitsa ciyembekezo cathu ca za m’tsogolo . M’masiku ano otsiliza , anthu a Mulungu amafunikila thandizo la kuuzimu la abusa acikondi . Lidzapitilizabe kugwila nchito mpaka Ufumu wa Mesiya utaononga adani a Mulungu , kuphatikizapo “ njoka , ” kufikila mabanja onse padziko lapansi atadalitsidwa . ( 1 Akor . Masiku ano , anthu ambili ‘ adziyeletsa ’ ndi ‘ kuyengedwa ’ ndipo ayamba kulambila koona . — Danieli 12 : 3 , 10 . Conco , Abulahamu analoŵela ca kum’mwela na banja lake kuyenda ku Iguputo . Ngakhale n’conco , panalinso zovuta zina . Ngakhale kuti mwina Davide anakhumudwa kuti sanakwanilitse cokhumba mtima wake , anacilikiza nchitoyo na mtima wonse . N’cifukwa ciani tikutelo ? Kumbukilani kuti ngakhale Akhristu ena amene anatumikila Mulungu kwa nthawi itali anagonja n’kukhala osakhulupilika . ( b ) N’cifukwa ciani tinganene kuti Mose anasankha zinthu mwanzelu ? Kumbukilani mmene iye anathetsela makhalidwe oipa amene anali ofala mu Sodomu ndi Gomora . Koma anam’limbikitsa . ( 1 Sam . ( Maliko 13 : 13 ) Conco , mofanana ndi Danieli , tiyenela kukhala pa ubwenzi wolimba na Mulungu wathu , Yehova . Cinanso , pewani mzimu wodzidalila , mwina poganiza kuti mumadziŵa zambili cakuti mungathe kusamalila mbali iliyonse popanda kufufuza malangizo mosamala . Kulimba mtima kwa abale athu m’mayiko ena kwacititsanso kuti tipambane milandu ina ngati imeneyi m’mayikowo . Poyamba , n’nali kuona ngati nikulota cabe . 11 : 39 , 40 ) Akhristu amene sali pabanja , amene akuseŵenzetsa umbeta wawo popititsa patsogolo “ zinthu za Ambuye , ” nawonso tiyenela kuwalimbikitsa na kuwayamikila kwambili . — 1 Akor . Pamene mtumwi Paulo anali ku Atene ku Girisi , anaona kuti kunali mafano ambili . Anthu anali kukhulupilila kuti mafanowo ndiye anawapatsa moyo . Madalitso anu ali pa anthu anu . ” — Sal . Kodi abale , monga amadela ndi akulu mumpingo , ayenela kucitanji akalandila malangizo a gulu la Mulungu ? Yehova adzakucilikizani mukadwala : Muzidalila Yehova kuti akusamalileni mukadwala . Iwo akumbukila zimene zinacitika paulendo wawo woyamba . Anayenda mtunda wa makilomita 32 pa njinga , kudutsa m’vikweza ndi m’misondo , dzuŵa lili phwee ! 1 : 26 , 27 ; Aef . Kucokela kwathu kukafika kumeneko , ulendo wa pa sitima unali kutenga maola anayi . 31 : 28 , 31 ) Komanso , Akhristu amene akupilila mokhulupilika cizunzo kapena matenda , amafunika kulimbikitsidwa . KODI vuto limeneli linayamba bwanji ? Iye anapita patsogolo mwamsanga , kenako anabatizidwa , ndipo panopa iye ndi mkazi wake Joyce , amasangalala kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu . Kuti mudziŵe za ciyambi ca lamulo la Karma , onani masamba 8 - 12 , m’kabuku kacingelezi kakuti What Happens to Us When We Die ? Pamene nkhondo yaciŵili ya padziko lonse inayamba , iwo sanavomele olo pang’ono kuloŵa usilikali . Komanso , si atsogoleli acipembedzo onse amene analudziŵa kuŵelenga na kulemba . Ndi ciani cina cimene Yohane analemba cokhudza wokana Kristu ? BUKU LACIWIRI Ilaria anakamba kuti : “ Tsiku lina madzulo , makolo anga anandiuza kuti ndioneka wosakondwela , ndipo anandifunsa cimene cikundivutitsa maganizo . ( Yos . 20 : 1 , 2 , 7 , 8 ) Popeza kuti Yehova ndiye analamula kuti pakhale mizinda yothaŵilako , tingafunse kuti : Kodi makonzedwe amenewa atiphunzitsa ciani za cifundo cake ? Willie ndi Liz Sneddon 8 : 3 . 1 : 28 ) Zikanakhala kuti Adamu na Hava anafa opanda ana , sembe colinga ca Mulungu cakuti padziko padzaze ana awo sicikanakwanilitsika . Ndiyo nkhani imene tidzakambilana mlungu wamawa . Mungakhale na cimwemwe cimene cimabwela cifukwa copatsa pa nthawi iliyonse . Mu 1999 , ine ndi Jenny tinalembanso buku lophunzitsa Cituvalu . Yehova amayamikilanso zimene acikulile amacita muutumiki wake . MAFUNSO OKHUDZA MBONI ZA YEHOVA AMENE ANTHU AMAFUNSA KAŴILIKAŴILI — N’cifukwa Ciani Simukondwelela Krisimasi ? Pamene mwapeza mpata , muziwalimbikitsa anzanu akusukulu kuti azidzifufuzila okha zinthu zimene afuna pa webusaiti yathu ya jw.org . Kodi Yehova watidalitsa bwanji kuti tikhale osangalala ? Kodi kukhala ndi mzimu wodzimana kumatanthauzanji ? Iye anaŵelenga mau a Yesu akuti : “ M’nyumba ya Atate wanga muli malo ambili okhalamo . . . . Aroma anali ndi miseu ya pamadzi yoposa 900 . 18 : 20 , 21 ; 22 : 12 ) Iye amakwanitsa kudziŵa zamtsogolo , koma amaganizilanso ufulu wathu wosankha . Coyamba , tiyeni tikambilane za colinga ca mizinda imeneyi . Mwacionekele , mungamuuze kuti timakhulupilila kuti Yehova ni Mlengi , amene anatipatsa moyo . Koma pakali pano , tidziŵa kuti Yehova amatikonda , ndi kuti amadziŵa mmene timamvelela tikamavutika . Mulungu “ Akwanilitse Zofuna Zanu , ” July Koma Naboti anati : “ Sindingacite zimenezo pamaso pa Yehova , kupeleka colowa ca makolo anga kwa inuyo . ” Tinali kuona monga ndi loto cabe . Pamene n’nali kugwila nchito m’Dipatimenti ya Utumiki , n’nafunsa mafunso apainiya amene anabwela kudzaona ofesi ya nthambi . Iwo anali kupita kukatumikila m’tauni ya Quebec , imene inali cimake ca citsutso . Ndipo mu 1939 , nkhondo yaciŵili ya padziko lonse inayamba . Zinali monga kuti nkhondo imeneyi inali kupitiliza nkhondo yoyamba . Popeza kuti kupanda cilungamo kwa conco kungacitike m’khoti iliyonse , Baibulo limacenjeza kuti : “ Uzitsatila cilungamo . Kodi n’zoona kuti kukhala pa nchito yapamwamba kungatibweletsele cimwemwe cokhalitsa ? Mavuto akabuka m’banja , okwatilana sayenela kuthetsa cikwati . Koma afunika kuyesetsa kukhala ogwilizana kwambili . Nikakumbukila izi , nimayamikila kuti Yehova anathandiza atate kulimba mtima . Onetsani kuti ndinu wokhulupilika . Amuna aŵiliwo sanadziŵe kuti maloto ao anacokela kwa Yehova , Mulungu wa Yosefe . Inde , tiyamikila ngako malangizo akuti tisaike kwambili patsogolo zinthu za “ thupi . ” Popeza maso anga aona Mfumu , Yehova wa makamu . Nditsikila kuli cete pakuti ndine munthu wa milomo yodetsedwa , ndipo ndikukhala pakati pa anthu a milomo yodetsedwa . ” ( Yes . ( Akol . 4 : 6 ) Komabe , cifukwa copanda ungwilo , nthawi zina tingakambe zinthu zimene tingacite nazo manyazi pambuyo pake . ( Yak . Koma woyang’anila ndende analengeza kuti : “ A Mboni za Yehova sakoka fodya . M’malomwake limalimbikitsa anthu kugwila nchito mwakhama . Ngati muyesetsa kucita zinthu mwaulemu ndi anthu , mwacionekele mudzakwanitsa kucepetsa nkhawa zanu . Mosiyana ndi mafumu ambili aumunthu , Yehova amaona atumiki ake kukhala banja lake . Amawakhulupilila kwambili ndipo amasangalala kuwapatsa ulamulilo ndi maudindo osiyana - siyana . ( Ŵelengani 1 Akorinto 4 : 17 . ) Kodi kuimba mokweza pamisonkhano mumakuona bwanji ? Koma ana ao aŵili anasangalala kucita zimenezo ndi makolo . Tiyeni tikambilane mafunso atatu ofunika aya : N’cifukwa ciani Yesu anakana kucilikiza magulu a zandale ? Cifukwa anaganizila mozama pa zimene anaŵelenga na “ kuzindikila tanthauzo lake . ” — Mat . Mayi wina wamasiye anati , “ Niona kuti cimene cimathandiza kuti cisoni cithe ndi zimene munthu amacita osati nthawi cabe . ” M’kupita kwa nthawi , Timoteyo anaphunzila kuthetsa manyazi amene anali kumulepheletsa kuuza ena uthenga wabwino wokamba za Yesu Kristu . M’kupita kwa nthawi , ndinapemphanso kuti ndizigwila nchito maola 48 pa mlungu . ( Nyimbo 4 : 1 - 5 , 8 , 9 ) Ngakhale kuti Solomo anayesa kukopa mtsikanayo mwa njila zosiyanasiyana , mtsikanayo anapitiliza kukonda m’busayo . Iye ayenela kuyesetsa kupeza thandizo kuti aleke cizoloŵezi coipa cimeneci . — Yak . Mungadziŵe zimenezi mwa kuphunzila mfundo za m’Baibo zili pa webusaiti ya www.jw.org . M’bale wokhulupilika ameneyu anakumana na zovuta mobwelezabweleza . Zoonadi , iye anacitilidwa zinthu zopanda cilungamo . Yehova ni Gwelo la mphamvu zopanda malile . ( Ŵelengani Mateyu 6 : 33 . ) Amene anafunsa funso limeneli ndi aneneli okhulupilika , Yesaya ndi Habakuku . ( Yes . ( b ) N’ciani cimatilepheletsa kupeza mtendele weni - weni masiku ano ? Ndiye cifukwa cake Paulo anawagogomezela kuti ‘ azikana mafunso opusa ndi opanda nzelu . ’ Iye anali kukonda kwambili kugwilitsila nchito mafanizo pophunzitsa . Zinthu zimenezi ndi : ( 1 ) mmene poyamba Petulo anakhulupilila kuti Yehova adzamuthandiza , ( 2 ) cimene cinapangitsa Petulo kuyamba kutaya cikhulupililo , ndi ( 3 ) cimene cinam’thandiza kulimbitsanso cikhulupililo cake . 4 : 32 ) Komanso , mneneli Yesaya anakambilatu za nthawi pamene anthu onse adzakhala na ufulu woseŵenzetsa cuma ca padziko lapansi . Kodi timacita kulambila kwa pabanja mlungu uliwonse ? ’ Pitilizani Kutumikila Yehova Mwacimwemwe , Feb . Apanso , n’nasiya malo amene n’nazoloŵela komanso abale na alongo n’colinga cakuti nikathandizile nchito pa Beteli . Pamene n’nali na zaka 14 , n’nayamba kupepa fwaka . n’zinthu ziti zimene anali kukamba ? Conco , Mboni zokhulupilika ku Mexico zinafunika kulimbikitsidwa mwauzimu . Kunena zoona , adani a munthu adzakhala a m’banja lake lenileni . ” — Mat . Atanyamula cida cimeneci , Davide anathamanga kuti akumane ndi mdani wake . Kuza ayenela kuti anali kuyang’anila cuma ca mfumu Herode Antipa . Kodi pangano latsopano limakhudza bwanji kudya zizindikilo za pa Cikumbutso ? Pambuyo pakuti Yesu wakhazikitsa mwambo wa Mgonelo wa Ambuye , iye na atumwi ake anaimba nyimbo zotamanda Mulungu . — Ŵelengani Mateyu 26 : 30 . Komabe , cifukwa cakuti ndinafuna kukondweletsa Yehova , sindinalole kulambila mizimu ya makolo . 103 : 21 . Kodi Mulungu ayenela kuloŵelelapo ndi kuletsa anthu kucita zinthu zoipa ? ( Yak . 3 : 2 ) N’zosavuta kuvomeleza mfundo imeneyi . Koma bwanji ngati m’bale watilakwila ? Mwacionekele , mtumwi Paulo anaganizila cocitika ici polemba kuti : “ Musaiŵale kuceleza alendo , pakuti potelo , ena anaceleza angelo mosadziŵa . ” Koma Mulungu sanawalole kuti akhalenso ‘ m’malo awo oyambilila . ’ NYIMBO : 153 , 104 Afunika kulabadila mwamsanga . Cikondi cawo cimakhala colimba ndipo amapilila . Malile amenewo ni citetezo . Mwacitsanzo , tili na ufulu woyendetsa motoka kupita kutali ku mzinda waukulu . Kodi inu kapena munthu wina wa m’banja lanu anacitilidwapo nkhanza ? Mizinda yambili monga Yerusalemu , inali kucinjilizidwa ndi zipupa zitali - zitali kuti adani asakwanitse kuloŵa mkati . Kodi cikumbumtima canga cimandicenjeza ndikayesedwa kuti ndionelele filimu imene muli zamalisece , kumwa mwaucidakwa , kucita zamizimu kapena imene imalimbikitsa ciwelewele ? ’ Ngakhale zili conco , tiyeni tipende lembali mozamilapo . TSAMBA 18 • NYIMBO : 46 , 63 Tiyenela kupeleka ndi mtima wonse cifukwa mwa kucita zimenezo , timaonetsa kuti ndife odzipeleka kwa Mulungu . Tingapeze mtendele weni - weni wa mumtima ngati timvela Yehova na mtima wonse . — Yes . M’Baibulo limenelo , munalinso zophophonya zambili , ndipo anaonjezelamo mavesi ena amene sapezeka m’mipukutu yakale . Tumabuku tumenetu tunali ndi zithunzithunzi ndi nkhani za “ Seŵelo , ” zimene zinapangitsa kuti Baibulo “ likhale monga buku latsopano . ” Misonkhano inali kucitikila ku nyumba ya m’bale wina , imene inali pamtunda wa makilomita 16 kucokela pamene tinali kukhala . Pambuyo pake , ‘ mpweya unalowa mwa anthuwo , ndipo iwo anakhala ndi moyo . ’ Pofuna kumveketsa bwino mfundo yakuti cikhulupililo ciyenela kuonetsedwa mwa nchito zathu , Yakobo anati : “ Monga mmene thupi lopanda mzimu limakhalila lakufa , naconso cikhulupililo copanda nchito zake ndi cakufa . ” — Yak . Ngakhale titaluza zinazake pofuna kukhazikitsa mtendele , Yehova adzatidalitsa . — Onani mau akumapeto . Zaka zambili zapitazo , iwo anali kusamalila atate ake Rose , amene anali kufunika kuwasamalila tsiku lonse . Zimalalikila m’mizinda ikulu - ikulu , m’midzi ya kutali , ndi kwa anthu okhala m’nkhalango , na m’mapili . KODI MUMAONA KUTI NDIMWE MUNTHU WACIMWEMWE ? Ndinamuuza kuti ndidzakufunsani ulendo wotsatila . Kodi kuukila kumeneku kusiyana bwanji ndi kuukila mwacindunji ? Panthawi imodzimodzi anaganizilanso za mmene akanalelela mwana wake Jimmy . Athandizeni kudziŵa kuti kutumikila Yehova ndi kopindulitsa kwambili . Iye anali kuuza Yehova zilizonse ngakhale zinthu zimene zinali kumuvutitsa maganizo . Kodi mwamuna wacikulile amene anali pa citsime ndani ? Mike anati : “ Tinaona kuti mau a Yesu olembedwa pa Mateyu 6 : 33 ndi oona . ” ( 2 Mbiri 14 : 1 - 7 ) Tiyeni tione zimene zinatsatilapo . Ngati Yesu nthawi zina anali kugona panja kukakhala kofunikila kutelo , ndiye kuti nafenso tiyenela kucita cimodzi - modzi mwacimwemwe ngati utumiki umene tapatsidwa ufuna zimenezo . ” Koma tifunika kukumbukila zimene zinacitikila Yehosafati . 4 : 9 ) Ponena za mphatso imeneyi , mtumwi Paulo analemba kuti : “ Kristu anafela anthu osapembedza Mulungu pa nthawi yoikidwilatu . Kodi inu mufuna kucita zimenezi ? Pankhaniyi , ganizilani za munthu woyamba , Adamu . Zimene ndinaphunzila zinali zotonthoza kwambili ” — Katlego , South Africa . 6 - 8 . ( Mat . 10 : 11 - 14 ) Zimenezo zidzacitika ngakhale kuti timafunsa mafunso oyenela , timakambitsilana nao bwino , ndi kugwilitsila nchito mafanizo omveka ndi osavuta . Iye analinso kukhulupilila kuti kulibe Mulungu ndi kuti zinthu zinacita kusandulika . Koma , asayansi azindikila kuti kacala kameneka n’kofunika kuti munthu azikwanitsa kuiimilila bwinobwino . Ndithudi , io ali paubale wamtengo wapatali ndi Mulungu . Colinga ca m’bale Knorr cinali cakuti Baibulo la Dziko Latsopano lithandize anthu mamiliyoni ambili kudziŵa Yehova . Akulu acikhiristu na makolo amaona kuti kuyamikila na kulimbikitsa munthu pomupatsa uphungu wa m’Baibo kumam’thandiza kuuseŵenzetsa . Tikufunilani zabwino zonse ! ” ( Ŵelengani Yoswa 20 : 4 . ) Ponena za nchito imene io akugwila modzipeleka ku Wallkill , anati : “ Kusiya umoyo wapamwamba kumafuna kulimba mtima , koma mukatelo mudzaona kuti mzimu wa Yehova umagwiladi nchito . ” Davide anadziŵa kuti mphamvu za munthu kapena zida sizinali zofunika kwenikweni . 19 : 27 ; 21 : 5 ; Agal . 3 : 24 , 25 ) M’zikhalidwe zina , kusunga ndevu zodulila bwino - bwino n’kololeka , ndipo kumapeleka ulemu . Iye anakamba kuti : “ Mwapemphelo ndimadalila thandizo la Yehova . ” Mwacionekele , tonse timakhudzika mtima tikaŵelenga nkhani za anthu amene Yesu anaukitsa . Ataphunzila kwa kanthawi , Kingsley analembetsa m’Sukulu ya Ulaliki . Kumvela ena cifundo kudzaticititsa ‘ kulankhula molimbikitsa kwa amtima wacisoni . ’ ( 1 Ates . Kukhulupilika kwathu kunabweletsanso madalitso ena . Ngati m’bale kapena mlongo wocokela dela lina wapeleka lingalilo , kodi mumakana ndi kunena kuti , ‘ Ife kuno timacita bwino kwambili kuposa kwanu ? ’ Ulosi wolembedwa pa Ezekieli 37 : 1 - 14 unanenelatu kuti anthu a Mulungu adzakhala akapolo , ndipo pambuyo pake adzamasulidwa . Kutsatila malangizo amenewa kudzakuthandizani kulemekeza Yehova ndipo mudzakhala acimwemwe . Iye anaganizilanso za mwamuna wolemala amene Paulo anacilitsa . Kodi ndi kuti kumene acinyamata angapeze thandizo popanga zosankha pa umoyo ? 23 : 15 , 16 ) Ndipo amapeza yankho loyankha Satana , amene amamutonza . Komabe , ndi mfundo zina ziti zamtengo wapatali zimene tingaphunzile m’buku la Levitiko ? ( Miyambo 14 : 15 ) Tili ndi cidalilo cakuti nkhani zotsatilazi , zikuthandizani kudziŵa kuti ndife ndani , timakhulupilila zinthu zotani , komanso kudziŵa nchito yathu imene timagwila . Zionetsa kuti onse aŵili anali kuona kuti kucita cifunilo ca Yehova ndiye kunali kofunika kwambili kuposa kukhutilitsa zilakolako zawo . N’cifukwa ciani tiyenela kulikonda kwambili Baibulo ? KUSAMALILA BANJA NDI KUTSATILA MFUNDO ZA M’BAIBULO ( Aef . 2 : 2 , 3 ) Monga mmene zilili na mizinda yambili masiku ano , nawonso mzinda wa Efeso unali wodzala na makhalidwe oipa . Conco , ciyelo ca akulu ansembe cimatithandiza kudziŵa kuti , aliyense amene akufuna kulambila Yehova ayenela kukhala “ woyela mumtima mwake . ” Kuti tipambane polimbana ndi Satana , tifunika kuyesetsa kulemekeza mphatso ya ukwati yocokela kwa Mulungu . Zaka 100 kapena kuposapo kumbuyoku , munthu anali kukhala na moyo zaka zocepa , ngakhale m’maiko olemela . Ndipo iwo sanazengeleze kubatizika . — Mac . 2 : 41 ; 9 : 18 ; 16 : 14 , 15 , 32 , 33 . Ngati mukhala na cidalilo pa zimene mumakhulupilila , kodi zingakuthandizeni bwanji kukhala omasuka kulalikila kwa ena ? Kodi Paulo anagwilizanitsa bwanji magazi ndi kukhululukidwa macimo ? Tingakhale ndi mtendele wa m’maganizo ngati tisiya zonse m’manja mwa Mulungu cifukwa iye ndi wamphamvu . Yehosafati anadalila Yehova ndi mtima wonse , ndipo anati : “ Maso athu ali pa inu . ” — 2 Mbiri 20 : 12 . Ndiponso popeza ndife opanda ungwilo , nthawi zina timaona zinthu molakwika . Yehova amafuna kuti mitu ya mabanja izisamalila mabanja ao nthawi zonse . Yesu analonjeza atumwi ake okhulupilika kuti akalamulila naye limodzi kumwamba . Tiyeni tiziyesetsa kufuna - funa mipata yothandizila ena . Mwacitsanzo , m’Baibulo mulibe malamulo amene amafotokoza mwacindunji zovala zimene tiyenela kuvala . Sitidziŵa zonse zimene Abele anali kuganiza ponena za mtsogolo , koma tidziŵa kuti iye anali ndi cikhulupililo cozikidwa pa lonjezo la Mulungu . 14 : 25 . ▪ Akulu , Kodi Mumakonda Kuphunzitsa Ena ? Kodi muyenela kuda nkhawa ? M’malo mokhumudwa na zophophonya za abale athu , tiyeni tikhale wotsimikiza mtima ‘ kuyang’anabe kwa Yehova Mulungu wathu , kufikila atatikomela mtima . ” — Sal . Rachel anali wamkali cifukwa ca mmene analeledwela . Ganizilani citsanzo ici : Dalaivala amadziŵa kuti nthawi ndi nthawi amafunika kuthila oilo watsopano mu injini kuti galimoto yake iziyenda bwino . Zimenezi zinanicitikila mu 1959 , nili m’ndende ina mumzinda wa Irkutsk , ku Russia . Liu lakuti “ mmodzi ” m’mau akuti “ Yehova mmodzi ” limatanthauzanso kuti colinga cake ndi zocita zake n’zodalilika nthawi zonse . 4 : 7 ) Mau a cinenelo coyambilila amene anatembenuzidwa kuti “ kuteteza , ” anali kugwilitsidwa nchito pokamba za asilikali . ( Yoswa 9 : 1 , 2 ) Pamene anali kumenyana ndi Aisiraeli , mafumuwo anali ndi mwai woona dzanja la Mulungu . Anakambanso kuti : “ Ukacita zimenezi , umacita cidwi kudziŵa kuti Mulungu amatikonda kwambili . ” Cifukwa cakuti mwacibadwa , ise tonse timafuna kuti anthu ena azitidziŵa . Iye anawatsimikizila mwacikondi kuti adzawathandiza kukhazikitsanso kulambila koona . Koma anawacenjeza mwamphamvu kuti adzawalanga ngati adzayamba kumulambila na mitima iŵili . Patangopita nthawi yocepa , Kristina anayamba kucita upainiya ndipo akusangalala . Kodi zinthu zimenezo n’ziti ? Ubatizo umaonetsa kuti munapanga lonjezo lapadela kwa Yehova . M’bale Atkinson anatipempha kuti tizipezeka ku misonkhano imene inali kucitikila kunyumba kwa M’bale wina , kutali pang’ono na kwathu . Ngakhale kuti matica a kusukulu kwathu anali kufuna kuti nikacite maphunzilo a ku yunivesiti , colinga canga cinali kukatumikila ku Beteli . ( Chiv . 7 : 9 ) Mwacitsanzo , Yefita , Yobu , ndi Rabeka anali kukambidwa kuti anali kuimila odzozedwa , pamene Debora ndi Rahabi anali kuimila khamu lalikulu . Ngati mufuna kuti Mulungu azikukhululukilani , inunso muzikhululukila ena ( Onani ndime 11 ) Komanso ubwenzi wathu ndi Yehova udzalimba ngako . Ndipo anthu amenewo akadzabwelela mumpingo , tiyenela kuwalandila mofanana ndi Yehova . TENGELANI CITSANZO CAO | YOSEFE ( a ) N’ciani cacititsa oyang’anila dela ena kukhala na nkhawa ? N’cifukwa ciani Mose anaona utumiki wake kukhala wofunika kwambili ? Koma ngati nthawi zonse mumacita zinthu mokhulupilika , pang’ono - pang’ono iwo adzayamba kukudalilani . ” — Brandon . ( a ) Kodi cikondi ca anthu okwatilana cimaphatikizapo ciani ? Amayi atakhutila kuti Mboni za Yehova zimaphunzitsa coonadi , anabatizika mu 1952 . Baibulo imatilangiza kuti : “ Usamafulumile kukwiya mumtima mwako , pakuti anthu opusa ndi amene sacedwa kupsa mtima . ” Nimadziŵa kuti munthu sakhuta na nthongo imodzi . Yehosafati anapanganso mgwilizano wina ndi anthu ena oipa . Izi n’zimene amayi ake a Maria anali kuganizila pamene anadzifunsa mafunso amene tawachula m’ndime yaciŵili . Makolo afunika kupenda kuti ni mu mpingo uti mmene ana awo angaphunzile coonadi mosavuta na kupita patsogolo , kaya ni mu mpingo wa citundu ca m’delalo kapena wa citundu cawo . Eduard Varter N’nali kuyesetsa kuti nisayambenso zizoloŵezi zanga , koma nthawi ndi nthawi anzanga amenewa anali kunisonkhezela kuti niyambenso . Nanga nifunika kuonetsa kwambili kudziletsa pa mbali ziti ? Komabe , kudzikonda kochulidwa pa 2 Timoteyo 3 : 2 si kwabwino ; n’kwadyela . Mateyu analemba kuti ‘ Mdyelekezi anatenga ’ Yesu ndi kupita naye ku Yerusalemu , ndipo “ anamukweza pamwamba pa khoma la mpanda wa kacisi . ” Tiyeni tikambilane mmene pangano lililonse limagwilizanilana ndi Ufumu , ndi mmene limagwilila nchito ponena za cifunilo ca Mulungu ca dziko lapansi ndi anthu . — Onani kamutu kakuti , “ Mmene Mulungu Adzakwanilitsila Cifunilo Cake . ” Angelo analengedwa ndi maumunthu osiyana - siyana , makhalidwe aumulungu , na ufulu wosankha zocita . ( Mat . 25 : 31 - 46 ) Mofananamo , kukwanilitsika koyamba kwa ulosi wa Ezekieli kumakhudza Akhiristu amene ali na ciyembekezo copita kumwamba . Colinga ca Yehova sicinali kungothetsa mavuto amene Yosefe anali kukumana nao , koma anali kufunanso kuti adzateteze mtundu wa Isiraeli mtsogolo . Pamene ndinali wacinyamata , ndinaphunzilako pang’ono coonadi ndi Mboni za Yehova Pamene Mfumu Davide analangidwa cifukwa cocita macimo aakulu , iye anavomeleza cilango ndipo anakhululukidwa . 10 , 11 . ( a ) N’cifukwa ciani mwana wamkazi wa Yefita anafunika kulimbikitsiwa ? Ndipo ngati ndinu kholo , mungapemphe mzimu wa Mulungu kuti ukuthandizeni kulanga ana anu mwacikondi osati mwaukali . Mwakamba zoona . Iye anakhulupilila Yehova ndi kumumvela “ tsiku lomwelo . ” — Genesis 17 : 10 - 14 , 23 . ( Aroma 8 : 28 - 30 ) Yehova anayamba kusankha odzozedwa Yesu ataukitsidwa . ▪ ‘ Anaona ’ Malonjezo a Mulungu Cifukwa ? Cifukwa cakuti cikhulupililo na cikondi zonse n’zofunika , Akhiristu olemba Baibo anawalembela pamodzi makhalidwe amenewa . Amapezeka kaŵili - kaŵili m’sentensi imodzi kapena m’ciganizo cimodzi . Kuthyola munthu miyendo kunali kucititsa kuti afe mwamsanga , ndiyeno anali kuikidwa m’manda Sabata lisanayambe m’madzulo . Baibo ya New World Translation of the Holy Scriptures — With References limaseŵenzetsa njila yolinganako pa mau ake amunsi . Abele ndi Enoki ndi ena mwa anthu amenewo . Kodi mumaona thandizo limeneli kukhala umboni wa cikondi ca Yehova pa imwe ? Komabe , Metusela anabeleka mwana dzina lake Lameki . N’cifukwa ciani mufunika kukhulupilila kuti ubale wanu na Mulungu udzakupatsani mphamvu ? Kodi dipo limeneli linakwanilitsa motani cilungamo ca Mulungu ? — 1 Tim . Nanga tidzaphunzila ciani m’nkhani yotsatila ? Cingelezi casintha kwambili kucokela pamene Baibulo la Dziko Latsopano linatulutsidwa koyamba . CHOONG KEON ndi mkazi wake Julie , a zaka za m’ma 30 , tsopano atumikila monga apainiya kwa zaka zisanu mumzinda wa Sydney ku Australia . N’zoona kuti ena palipano mikhalidwe siwalola kucita utumiki wanthawi zonse . Sanali kukondwela ndi anthu amene anali kupeputsa zimene Baibulo imaphunzitsa mwa kulemekeza miyambo ya anthu . ( Aroma 15 : 5 ) Ndi yekhayo amene amadziŵa bwino kwambili mavuto athu , mmene timamvelela , ndi mmene tinakulila . Ni mavuto ati amene anthu othaŵa kwawo amakumana nawo ( a ) pothaŵa ? Ndipo cifukwa ca lonjezo limeneli , mwana wake wamkazi mmodzi yekhayu sakanakwatiwa kuti amubelekele adzukulu . Mulimonse mmene iye akanasankhila , zotulukapo zake zikanakhudza umoyo wake wonse . M’masiku a Mfumu Yehosafati , anthu a Mulungu anayang’anizana ndi “ khamu lalikulu ” la adani ocokela m’madela ozungulila . Kucokela pamene Yehova analenga anthu , iye wakhala akuwapatsa malangizo omveka bwino . Mwa njila imeneyi , Yehova anasonyeza kuti anali kukonda kwambili Adamu ndi Hava . Kodi Davide anayamba kulaka - laka kukhala mfumu ? Kuphwanya lonjezo la cikwati n’kunamiza Mulungu , ndipo Mulungu amadana ndi anthu abodza . ( Lev . 19 : 12 ; Miy . ( Ezara 1 : 2 , 3 , 5 ) Iwo anacoka m’dziko limene anajaila kukhalamo n’kupita kukakhala m’dziko limene ambili a iwo anali asanalionepo . Ndife okondwa kwambili kuti Yehova amatipatsa mphatso zamtengo wapatali kwaulele ngati buku limeneli . ” Kodi cifukwa cacikulu cokhalila na zolinga zauzimu n’citi ? VUTO : Mwina mungaganize kuti kuika malamulo atsopano kungathandize kuthetsa ziphuphu . Zimenezi zimaonetsa kuti mumawakonda . ” Ndipita kukaukila anthu amene akukhala mwabata , popanda cowasokoneza . Mwacitsanzo , ngati tikukambilana za Ufumu wa Mulungu ndi munthu winawake , sitiyenela kukamba kuti tikugwilizana kapena sitikugwilizana ndi mfundo ya cipani cinacake kapena mtsogoleli winawake . Kodi mudzacita ciani ngati mwayesedwa kuti musakhale wokhulupilika kwa Yehova ? 9 , 10 . ( a ) Malinga ndi Deuteronomo 4 : 5 - 8 , kodi Cilamulo cinasiyanitsa bwanji Aisiraeli ndi anthu ena ? Ni ufulu wanji umene Adamu na Hava anali nawo ? Mulungu amayankha panthawi yake . Coyamba , mungayambe kuphunzila cinenelo ndi cikhalidwe ca anthu a kudzikolo . Cikondi cimeneci cimayendela mfundo za m’Baibo komanso cimaphatikizapo ubwenzi na cifundo . Ngati ngamila zonse 10 zinali ndi ludzu kwambili , ndiye kuti Rabeka anagwila nchito yotunga madzi kwa maola ambili . Tikanangomudziŵa kuti ndi munthu amene anagawanitsa Nyanja Yofiila kapena munthu amene analandila Malamulo Khumi . Kufunsa mafunso makolo anga a Ron ndi a Estelle pa msonkhano wacigawo mu 2014 , ku Townsville , ku Australia N’ciani cingakuthandizeni kuti mujaile ? ( Yohane 5 : 28 , 29 ; Chivumbulutso 21 : 3 , 4 ) Ndiyeno , onse adzakamba mau a mtumwi Paulo akuti : “ Imfa iwe , kupambana kwako kuli kuti ? Coyamba , tiliguyo anali kusakanizidwa ndi madzi , kuusinja ndi kuuyanika pa dzuŵa . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Aliyense payekha ayese nchito yake , kuti aone kuti ndi yotani . Koposa zonse , Yehova anali kuona citsanzo cabwino ca Timoteyo . “ Kungomva kulila kwa galimoto iliyonse imene inali kudutsa mkwiyo wanga unali kuonjezeka . Iye anasankha atumwi ake 12 kuti ayale maziko a nchito ya padziko lonse . Pambuyo pake anaphunzitsa ophunzila ake 70 . N’cifukwa ciani Mose anapeleka malangizo kwa Aisiraeli ? Ni zitsanzo ziti za atumiki a Mulungu amene sanataye cikhulupililo ? Nanga n’ciani cinawalimbikitsa kucita zimenezo ? ( Aroma 5 : 12 ) Mau a Mulungu amachula imfa kuti “ mdani . ” Kuthandiza ofooka kumabweletsa madalitso otani ? Komanso iye atafa , ufumu wa Isiraeli unagaŵikana moti mafumu obwela pambuyo pake anakumana na mavuto ambili kwa zaka zoculuka . — 1 Maf . N’nacita cidwi kudziŵa kuti aliyense akhoza kukhala na ciyembekezoci , ngati ayesetsa kutsatila miyezo ya Mulungu ya makhalidwe abwino ya m’Baibo . ( Ŵelengani ) Ndiyeno , tidzakambilana zitsanzo zina za m’Malemba za anthu amene Yehova anawathandiza m’njila imene iwo sanali kuyembekezela . Kodi Yesu anacita ciani ataona cikhamu ca anthu amene anali kumutsatila ? Amapatsidwanso utumiki wocezela maofesi a nthambi monga oimila likulu la Mboni za Yehova . Anthu amene amalephela kulamulila mkwiyo nthawi zambili amakhala osakondwa . 147 : 19 , 20 ) Malinga ndi Cilamulo , anthu ena anaikidwa kukhala ansembe . Kaya yankho lanu ndi lotani , tiyeni tikambilane zifukwa zitatu zamphamvu zimene zimatipangitsa kukhulupilila kuti cifunilo ca Mulungu cidzacitika posacedwapa padziko lapansi . APAKAVALO AONEKELA Kuti tiyamikile “ mphatso yangwilo ” imeneyi tiyeni tione mmene ikwanilitsila mfundo zimene tinakambilana m’nkhani yapita . 5 : 33 ) Ngati a m’cikwati oopa Mulungu akhala mogwilizana , kukwesana m’banja kumacepa , ngakhale kuthelatu . Yehova atalenga anthu , sanawapatse ufulu wolamulila anzao . Thupi la Yesu linaikidwa m’manda osemedwa m’thanthwe , ndipo anatseka khomo la manda amenewo ndi cimwala cacikulu . Inde , n’zotheka . ( Aroma 3 : 21 - 26 ) Ndithudi , Yesu wacita mbali yaikulu potithandiza kuyandikila Mulungu . Abulahamu sanali kudziŵa nthawi imene mwana wake adzaukitsidwa n’kukhalanso na moyo . Cikondi ceniceni ndiponso mgwilizano umene uli pakati pa atumiki a Yehova umawadziŵikitsa kuti ali m’cipembedzo coona . ALIYENSE ADZAKHALA NA CAKUDYA COKWANILA : “ Padziko lapansi padzakhala tiligu wambili . Pamwamba pa mapili padzakhala tiligu woculuka . ” — Salimo 72 : 16 . Ndiyeno icekeni pakati na kum’patsa kambeu kake . Conco , makolo amalephela kudziŵa maganizo a ana awo ndi mmene amvelela . ” Limakamba zimenezi buku lakuti , Breaking the Code . Tsiku lina , patapita mwezi umodzi , tinalema ngako pambuyo poyenda ku nyumba ndi nyumba kukacititsa maphunzilo a Baibo m’nyengo yotentha imeneyo . Bukuli limafotoza kuti zimenezi zakhala zikucitika mwapang’onopang’ono . Limati : “ Anthu akhala akudula mitengo makamaka kuti alambule malo olimapo ndi odyetsela ziŵeto , komanso kuti apezeko zomangila ndi nkhuni . ” — Plants of the Bible . n’nafunsa Izak Marais . Koma n’nayamba kuphunzila zinthu zina zimene zinasintha kwambili umoyo wanga . Motelo , wacinyamata wamng’ono wokhwima mwakuuzimu amene wabatizidwa , akhoza kucita zinthu zoyenela ngakhale kuti makolo ake kapena anthu ena acikulile ali kutali . — Yelekezelani ndi Afilipi 2 : 12 . Ndi zinthu ziti za m’dzikoli zimene timagwilitsila nchito ? NJILA YOTHETSELA VUTOLI : Malamulo a Ufumu wa Mulungu ndi apamwamba kwambili kuposa malamulo a maboma a anthu . Safunika kusankhana ndaŵa otsatila onse a Khristu ni “ munthu mmodzi . ” — Akol . A Zulu : Cabwino , koma onani kuti lembali lanena kuti Ufumuwu “ udzakhalapo mpaka kalekale . ” Mogwilizana ndi mau a Yesu , munthuyo ‘ amadzikana yekha . ’ Amasiya moyo wodzikondweletsa yekha , ndipo amalonjeza kuti adzaika patsogolo zofuna za Mulungu mu umoyo wake . ( Mat . Munthu amene ananyamula kacikwama konyamulilamo inki akuimila Yesu . Mlongo wina dzina lake Hilda Padgett * anati : “ Limenelo linali pempho locokela ku likulu limene ambili aife tinali kuliyembekezela . Posapita nthawi , panakhala zotulukapo zabwino ngako . ” Ndiye cifukwa cake anauza Yoswa kuti aziŵelenga buku la cilamulo ndi “ kusinkhasinkha , ” kutanthauza kuliŵelenga capansipansi . Koposa zonse , tikamvela malamulo a Yehova , kuphatikizapo lamulo lakuti tizilalikila , iye adzakondwela kwambili ndipo adzatidalitsa . David anali na khalidwe loipa ndipo anali kukamba mau oipa kwa ena . ( Genesis 40 : 17 ; 1 Samueli 8 : 13 ; Yesaya 55 : 2 ) M’nthawi ya Yeremiya , ku Yerusalemu kunali “ mseu wa ophika mkate . ” Ndipo m’nthawi ya Nehemiya , nsanja ina ya kumeneko inali kucedwa “ Nsanja ya Mauvuni . ” — Yeremiya 37 : 21 ; Nehemiya 12 : 38 . Iye anati : “ Kuti ndidzatuluke m’ndende muno . ” ( Genesis 4 : 6 , 7 ) Koma Kaini sanalandile thandizo la Yehova ndipo anavutika kwambili ndi zotsatilapo zake . Kodi mumayamikila Yehova makamaka cifukwa ca ciani ? Sanapeze nchito . Tingakambe ciani ponena za mmene timadziŵila mkazi ndi mbeu yake ? Komabe , Aisiraeli analephela kumvela malamulo amenewo . Nthawi zina zimavuta kumvetsa mavuto amene ena akukumana nao . Mzimu woyela ungatiumbe m’njila zosiyanasiyana . Nthawi zina , akhoza kumasinthana kuyendetsa , ndipo m’kupita kwa nthawi , tateyo amasiyila mwana wake kumayendetsa nthawi zambili . Mfundo zitatu za m’Baibo zimene takambilana zingakuthandizeni pamene mufuna kusankha nchito . Acicepele ali ndi mphamvu yocita zambili mu utumiki wa Yehova . Kodi imwe mudzacita ciani ? Iye anayankha motsimikiza kuti : “ Inde M’bale , ndakhala ndikuyeseza kwa maulendo 30 . ” ( Miyambo 18 : 21 ) Koma kodi zimenezi zitanthauza kuti tiyenela kukhala duu osakamba ciliconse cifukwa coopa kukamba mau oipa ? Monga mmene kum’mawa kwatalikilana ndi kumadzulo , momwemonso , watiikila kutali zolakwa zathu . ” Nchito imene Mulungu amapatsa atumiki ake imasiyanasiyana malinga ndi mmene cifunilo cake cikukwanilitsidwila . Yesu anati : “ Pitani mukaphunzitse anthu . . . kuti akhale ophunzila anga . . . ndi kuwaphunzitsa . ” Kapena mungawapatseko zakudya , kuwathandiza nchito za panyumba , ndi kuwanyamula pa galimoto popita kumisonkhano . Kapenanso mungawapemphe kuti muyende nao mu utumiki wa kumunda . tizikhala bwino na ena ? Koma umphawi uli ponse - ponse , ngakhale m’maiko olemela ulimo . N’nabadwila m’dela lokongola la Ciudad Mante , m’tauni ya Tamaulipas , ku Mexico . Mungalimbikitse ena mwa kuwasimbila zocitika zimene mwasangalala nazo potumikila Mulungu . Kuti mudziŵe zambili za nchito yomasulila ku Samoa , onani Buku Lapacaka lacingelezi la mu 2009 , tsamba 120 - 121 ndi tsamba 123 - 124 . Iwo amacita zimene angathe kuti asabwelele ku umoyo wakale wokonda zinthu zakuthupi ndiponso wodzikonda . Ngakhale kuti Mulungu anakambapo ndi anthu kupitila mwa angelo , iye satilola kuwalambila kapena kupemphela kwa iwo . — 1 Akorinto 13 : 1 ; Chivumbulutso 22 : 8 , 9 . KHALANI WODZICEPETSA : “ Nzelu zimakhala ndi anthu odzicepetsa . ” Conco , “ mtendele wa Mulungu ” ungapambane vuto lililonse limene mungakumane nalo . Mwacitsanzo , ganizilani za katswili wina wa zacipembedzo wa m’zaka za m’ma 1300 C.E . , dzina lake John Wycliffe . Amuna acikulile ndi acicepele amavala matayi ndi majekete . Azimayi ndi atsikana amavala masiketi aatali bwino . . . oyenelela koma amakono . ” Mkati mwa mlungu ndinali kupita ku mapwando , kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza bongo ndi kucita ciwelewele . Yesu anapemphelela ophunzila ake kuti : “ Sindikupempha kuti muwacotse m’dziko , koma kuti muwayang’anile kuopela woipayo . ” Kuuza mwana wanu mau akuti , “ Ungakambe nane nthawi iliyonse ” si kokwanila . Tinaipemphelela nkhaniyi ndi mkazi wanga , ndipo tinakambilana ndi makolo athu okalamba kuti timvele maganizo awo . Patapita zaka ziŵili , sitima ya Titanic inasweka n’kumila m’madzi . ( Mat . 13 : 41 - 43 ) Conco , ino ndiyo nthawi yakuti anthu amene akuyembekezela kudzaweluzidwa monga nkhosa athandize abale a Kristu mokhulupilika . Baibo imakamba kuti anali ‘ kuona ena onse ngati opanda pake . ’ — Luka 18 : 9 - 14 . kupanga zosankha pamene sitili otsimikiza ? Kodi angelo anam’thandiza bwanji Yesu atangobatizika ? Onani tanthauzo lina la cikondi limene Paulo anafotokoza . afunika kujuŵa nthambozo . Ngakhale n’conco , pali zimene tingaciteko kuti titeteze thanzi lathu . 4 : 13 ; Maliko 6 : 3 ) Ngakhale zinali conco , ophunzila ake anabwelako ali ndi cisangalalo cacikulu . N’zomvetsa cisoni kuti anthu ambili akuvutika na cisoni cotele . APAINIYA A NTHAWI ZONSE Amatimvelelanso cifundo ngati tikumana ndi mavuto a zacuma , kapena tikalephela kucita zambili mu utumiki cifukwa ca thanzi lathu kapena kuvutika maganizo . NKHANI YA PACIKUTO | MMENE MULUNGU AMAONELA KUKOKA FODYA Koma acicepele kapena obatizika catsopano amafuna kuti azitengeko mbali m’zocitika za pa mpingo . Zolemba zakale zofotokoza mbili ya Ayuda zionetsa kuti amalonda a pakacisi anali kudyela masuku pamutu makasitomala awo mwa kuwachaja mitengo yokwela kwambili . Timaonetsa kuti timamuyamikila Yehova mwa kudzipatulila kwa iye na mtima wonse . ( Onani pikica pamwambapa . ) ( b ) Kodi aliyense adzamvela bwanji dzikoli likadzawonongedwa ? Mungagulitse , kupatsa ena , kapena kutaya zinthu zimene munaleka kuseŵenzetsa . Kwa zaka zambili , ine ndi Jenny , tinalandila mautumiki osiyanasiyana mu zilumba za ku Pacific . Samueli ataleka kuyamwa , Hana anapita kukam’peleka ku cihema , mogwilizana na lumbilo lake . Baibulo limanena kuti iye “ anakagona pabedi lake n’kutembenukila kukhoma , ndipo sanadya cakudya . ” Kim sanali kukambako nkhani zimenezi cifukwa sanali kucitako khalidwe loipalo . Mbali yomaliza ya lemba limene ndimakonda kwambili limati : “ Kuti ndilengeze za nchito zanu zonse . ” Mwina Mariya anadela nkhawa kuti , ‘ kodi anthu akadziŵa kuti ndili ndi pakati adzandiona bwanji ? Tsopano ku Tulun kuli mpingo umene uli na ofalitsa oposa 100 . Claire ( pakati ) Yesu tsopano akutsogolela nchito yolalikila ya otsatila ake oona . N’cifukwa ciani tiyenela kutengela Yesu ? M’pempheni kuti iye ndi banja lake pamodzi ndi banja lanu mukalalikile m’gawo limene kulibe wolalikila kapena limene silifoledwa kaŵilikaŵili . Ndikamamuyamikila m’pemphelo , ndimakumbukila zinthu zimene wandicitila . ( Aroma 5 : 12 ) Zimenezi ziyenela kutithandiza kuseŵenzetsa mwanzelu ufulu wathu wosankha zocita , komanso mosapitilila malile amene Yehova anatiikila . Ndipo Mulungu amene dzina lake ndi Yehova , walonjeza kuti “ olungama adzalandila dziko lapansi , ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya . ” Iye anasankha kuti tiziphunzila tsiku lililonse , ndipo anali kukonzekela bwino cakuti m’mwezi umodzi cabe tinatsiliza kuphunzila buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa . Atate anga anali mmisili wazitsulo , ndipo amai anga anali mlimi . Ngakhale kuti muli ndi ulamulilo pa ana anu , mukhozanso kukhala bwenzi lao . Mwana amafunika kumufotokozela zinthu pang’ono ndi pang’ono kuti akakhutile . ” Monga mmene Mulungu anathandizila Yosefe , iye angatithandize kuti tisataye mtima koma kuti tikhalebe ndi ciyembekezo colimba . — Aroma 12 : 12 ; 15 : 13 . Masiku ano , zinthu zoopsa zimenezi zimacitika kaŵili - kaŵili ndipo zimapha anthu ambili kuposa kale lonse . Iye anayamba kuganiza kuti nchito ya pa fakitaleyo ni kupanga mitambo . Iye anauza atumwi ake kuti : “ Mupitiliza kukhala mabwenzi anga mukamacita zimene ndikukulamulani . ” Nkhani ina yofotokoza za kusamalila okalamba inati : “ Ngakhale kuti kukambitsilana nkhani yosamalila okalamba kungakhale kovuta , banja likakambilana pasadakhale njila zocitila zimenezi lingasamalile bwino mavuto amene angabwele . ” Mwacionekele , ise tonse timafunitsitsa kuonetsa kuti timamuyamikila Yehova potipatsa mwayi wokhala anthu ake . Kodi n’napezeka bwanji m’vuto limeneli ? 3 : 16 , 17 ; 1 Akor . ( a ) Kodi mphatso ya ufulu wosankha zocita inamusiyanitsa bwanji Adamu ku zolengedwa zina mu Edeni ? ( Miy . 21 : 5 ) Timafunika kupatula nthawi yoganizila mosamala kwambili mfundo zosiyana - siyana zokhudzana ndi cosankha cimene tifuna kupanga . Tikacita conco , ndiye kuti zinthu zidzatiyendela bwino . N’tangomuona Maria , n’namukonda kwambili . Zida zonse zankhondo zidzawonongewa Katswili wina , James Parkes , analemba kuti : “ Ayuda . . . anali kuloledwa kucita miyambo yawo . Kodi ndine wokonzeka kukhululukila amene anilakwila ? ’ pamenepo mudzawauze kuti , ‘ Umenewu ndi mwambo wopeleka nsembe ya Pasika kwa Yehova , amene anapitilila nyumba za ana a Isiraeli mu Iguputo pamene anali kupha Aiguputo ndi mlili , koma anapulumutsa mabanja athu . ’ ” ( Eks . Kodi cikumbumtima cathu cimafanana bwanji na kampasi ? Pofika mu 1915 , Nsanja ya Mlonda inayamba kusindikizidwa mu Cipolishi mwezi uliwonse , ndipo The Golden Age ( tsopano imachedwa Galamukani ) inayamba kupezeka m’cineneloco mu 1925 . Ophunzilawo anaona kuti pafunika kukhala atumwi 12 . Ndidye cakudya cimene ndikufunika kudya . ” N’ciani cimene tiyenela kukumbukila tisanauze munthu malangizo okhudza thanzi kapena ifeyo tisanatsatile malangizo amene tapatsidwa ? ( Mateyu 24 : 14 ) Nchito yolalikila imeneyi ndi yofunika ndipo kuyambila kale nchitoyi yakhala yosiyana kwambili ndi zimene zipembedzo zambili zimaphunzitsa . Mwina amaopa kuti mau awo angamveke kwambili kuposa a ena onse . Kodi makolo ena anaphunzila ciani panthawi ya nkhondo ku Balkans ? Conco inuyo ndi mbadwa zanu musankhe moyo kuti mukhalebe ndi moyo . ( Yobu 2 : 11 ; 22 : 1 , 5 - 10 ) Komabe , Yobu anakhalabe wokhulupilika . Tingacite zimenezo mwa kuŵelenga zinthu zimene anacita ndi kuphunzitsa , ndiponso kum’tsatila mosamala kwambili . Nanga n’cifukwa ciani tili na moyo ? Mpaka lomba , tonse tikuvutika kaamba ka cosankha coipa cimene Adamu anapanga . Kucita phunzilo laumwini mwakhama kungakuthandizeni kuyankha mafunso , kuthetsa zikaikilo zimene mungakhale nazo , ndi kulimbitsa cikhulupililo canu . July Conco apite . ” ( 2 Mbiri 36 : 23 ) Izi ziyenela kuti zinawalimbikitsa kwambili Aisiraeli amene anali kukhala ku Babulo . Mungaseŵenzetsenso zakumapeto mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika , kapena kabuku kakuti Buku Lothandiza Pophunzila Mau a Mulungu . Ndinayamba kuleka pang’onopang’ono kukoka fodya , mpaka ndinalekelatu . ” Sikutanthauza kucepetsa colakwaco , kapena kuciona monga kuti sicinacitike . Cimodzi mwa zolinga za magazini a Nsanja ya Mlonda ndi ‘ kulimbikitsa anthu kukhulupilila Yesu Kristu amene anatifela kuti tikapeze moyo wosatha ndipo panopo akulamulila monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu . ’ Ku nkhondoko , Yehosafati anapulumuka ngakhale kuti anatsala pang’ono kuphedwa . Cifukwa codalila luso lake , mkulu angayambe kumasamalila maudindo a mpingo , monga kukamba nkhani , osayamba wapemphela n’komwe kwa Yehova . ( Mateyu 28 : 20 ) Conco Yesu analonjeza otsatila ake kuti iye adzawatsogolela pa nchito yolalikila , ndipo adzawathandiza kulalikila padziko lonse lapansi . N’talandila cilolezo , n’nafika ku Paraguay mu March 1959 . Panthawiyo , anthu omwe iye anali kulamulila anali “ kukhala mwabata ” ndi mwamtendele . Zinthu zinali kuwayendela bwino ndipo anali “ kudya , kumwa ndi kusangalala . ” — 1 Mafumu 4 : 20 , 25 . Ena afika mpaka posiya coonadi . Koma panali anthu ena ocepa amene anati cicitike cicitike , sadzamuyopa Babulo Wamkulu ! Yesu anazindikila kuti mayiyo analapa , ndipo anadziŵanso mmene akanamvelela akanamukalipila . ( Afil . 1 : 10 ) Muziika patsogolo zinthu zimene Mulungu amaona kuti n’zofunika kwambili . Mwacitsanzo , pa nkhondo yaciŵili ya padziko lonse , asilikali anasonkhanitsa abale athu okwanila 160 a zaka zosafika 45 , amene anali m’ndende zonse za ku Hungary ndi kuwaika pamalo amodzi . Kodi izi si zimene tinalonjeza kuti tidzayamba kucita ? ( 1 Mafumu 8 : 41 - 43 ) Koma m’kupita kwa nthawi , Yesu anapeleka lamulo limene lili pa Mateyu 28 : 19 , 20 . ( 2 Mbiri 16 : 9 ; Yobu 1 : 8 ) Yehova na Yesu amayamikila ngako zimene timacita pocilikiza zinthu za Ufumu , ngakhale kuti sitingacite zambili cifukwa ca mmene zinthu zilili pa umoyo wathu . Mabuku a Mateyo ndi Maliko amanena kuti : “ [ Mwana wa munthu ] adzatumiza angelo ndipo adzasonkhanitsa pamodzi osankhidwa ake kucokela kumphepo zinai , kucokela kumalekezelo ake a dziko lapansi kukafika kumalekezelo a m’mlengalenga . ” Kodi mumakuona kuti n’kocititsa manyazi ? Mateyu 28 : 19 , 20 Kodi n’ciani cimene tingacite kuti tilimbitse mgwilizano pakati pathu ? Cingatithandizenso kupilila mavuto . Baibulo siifotokoza kuti Nero anaweluza yekha mlandu wa Paulo kapena anasankha munthu wina kuti amve dandaulo la Paulo ndi kum’pelekela lipoti . 21 : 43 . Koma imwe munanimanga . Ngakhale kuti tifunika kukhala okoma mtima kwa anthu amene satsatila malamulo a Mulungu , tiyenela kusamala kuti anthuwo asakhale mabwenzi athu apamtima . Dalitso limene Yakobo analandila linali kusintha dzina lake kukhala Isiraeli . Ca pakati pa zaka za m’ma 1960 , banja lina la Mboni locokela ku Latvia limene linaphunzilila coonadi m’dela la kumwela kwa Bronx , linasamukila m’gawo la mpingo wathu . Anthu ena amaphunzila coonadi ca m’Baibo ndi kuona kufunika kobatizika ali acikulile , ndipo ena anabatizikapo ali na zaka zopitilila 100 . Mwa ici , Yehova analanditsa Rehobowamu na mzinda wa Yerusalemu m’manja mwa Sisaki . — 2 Mbiri 12 : 5 - 7 , 12 . Amalola mkwiyo na kukhumudwa kuononga maubwenzi awo ndipo zimenezi zimalengetsa munthu kudzipatula na kusungulumwa Ngati m’bale kapena mlongo wapeza munthu amene m’kupita kwa nthawi wakhala wophunzila , tonse timakondwela cifukwa timagwilila pamodzi nchito yofufuza anthu oona mtima . Ophunzila a Yesu safunika ‘ kukhala ndi moyo wongodzisangalatsa okha , koma wosangalatsa amene anawafela n’kuukitsidwa . ’ — 2 Akor . Nthawi ina , Yesu anakamba za mnyamata wina amene anacoka pakhomo pa atate wake ndi kuononga colowa cake conse mwa kulowelela m’makhalidwe oipa . Ngakhale acicepele anali kukamba nkhani papulatifomu . Conco , anayambanso kuphunzila Baibo , ndipo m’kupita kwa nthawi anayenelela kukhala wofalitsa uthenga wabwino . 13 , 14 . ( a ) N’ciani cinathandiza Mose kuti ayenelele nchito imene Yehova anam’patsa ? Kugwilitsila nchito magazi a nyama kumene mkulu wa ansembe waciisiraeli anali kucita pa Tsiku la Mwambo Wophimba Macimo , kumatithandiza kudziŵa mmene Mulungu amaonela magazi . ( Ŵelengani Mateyu 24 : 33 - 35 ) Pamene Yesu anakamba kuti “ m’badwo uwu , ” iye anali kunena za magulu aŵili a odzozedwa . ( Mateyu 24 : 33 ) Dzifunseni kuti , ‘ Ndi liti pamene zinthu zonse zochulidwa m’Baibulo ( 1 ) zinacitika padziko lonse lapansi , ( 2 ) zinacitika panthawi imodzi , ndi ( 3 ) zinaipilaipilabe ? ’ Jason , amene akutumikila pa ofesi ya nthambi ina mu Africa muno , wakhala muutumiki wa nthawi zonse kwa zaka zoposa 30 . Conde ilandileni . ’ Ndipo cikondi cimeneci cidzakhalapo kwamuyaya . ( 1 Timoteyo 6 : 19 ) Palibe buku lina lililonse limene lingatiuze za tsogolo labwino ngati limeneli . * M’malo mwake , iye “ anakhala pansi kudzanja lamanja la Mulungu . Kuyambila pamenepo , akuyembekezela kufikila pamene adani ake adzaikidwe monga copondapo mapazi ake . ” — Aheb . Mwamuna wa m’banjali , dzina lake Vicent anati : “ Zimene n’naŵelenga m’Baibo zinanithandiza kucita zinthu mwacikondi polimbana ndi mavuto m’banja lathu . Ni zocitika zakale ziti zimene zinathandiza Akhristu kukhala na cikhulupililo cakuti akufa adzauka ? Pamene ikuyendetsa hachi yake , Mfumu yamangilila lupanga m’ciuno mwake . ( Akolose 1 : 15 - 17 ) Motelo , Yehova analemekeza kwambili Mwana wake mwa kumugwilitsila nchito polenga zinthu ndi kufotokozela ena za udindo wake waukulu . 1 : 27 , 28 . Ngati tikukumana ndi vuto linalake , tizigwilitsila nchito nthawi imeneyo kuyandikila kwambili Yehova . Atapita patsogolo m’kuphunzila kwake , anazindikila kuti Mulungu anapatsa iye udindo wolela mwana wake , na kum’phunzitsa kulambila Yehova . ( Sal . 127 : 3 ; Miy . Pamene m’bale wina wa zaka za m’ma 60 anafunsidwa cifukwa cake amakhulupilila kuti wapeza coonadi , iye analoza kwa Yesu Kristu mwa kufotokoza kuti : “ Tinaphunzila umoyo ndi utumiki wa Yesu mwakhama , ndipo timatsatila citsanzo cake . Sititanthauza kuti acinyamata azingoyendela njila zakale ayi . Koma asamafulumile kukana uphungu wa acikulile . Kodi fanizo la mwana woloŵelela limatanthauza ciani ? 10 , 11 . ( a ) Ni fanizo liti limene mungakonde kuseŵenzetsa kuti muthandize mwana wanu kukulitsa cikhulupililo mwa Mulungu ? Christian anati : “ Tsiku lina pa Kulambila kwathu kwa Pabanja , tinakambilana nkhani ya zosangulutsa . Mosasamala kanthu za kumene timakhala , timamvela malamulo ndipo sitiloŵelela m’ndale za dziko . Mwacitsanzo , olambila oona amasangalala ndiponso amalimbikitsana akasonkhana kuti alambile Yehova . ( Sal . Pa cikondweleloco , Farao anaweluza atumiki ake aŵiliwo . Iye anapha mkulu wa ophika mkate ndi kubwezela pa nchito mkulu wa wopelekela cikho uja , monga mmene Yosefe anakambila . Munthu uyu ndi mwana wa m’bale wanga . Tiyeni tikambilane mmene anali kucitila pomvetsela ndi zimene anali kukamba . Komatu palibe ngakhale imodzi imene idzagwa pansi Atate wanu osadziŵa . Ndipo akalibe kukhala mfumu , iye anafunika kukumana na mavuto na kuphedwa . Njila yolemba mau kaŵili ndi kuwalinganiza ndi amene ali pa kompyuta inacititsa kuti kulakwitsa kucepe . Akakonza mmene bukulo lidzaonekela , anali kutitumizila kupyolela pa melo kuti tilione . Pakuti Mulungu anati : ‘ Sindidzakusiyani kapena kukutayani ngakhale pang’ono . ’ Ambili ni osauka kapena akuvutika cifukwa ca nkhondo ndi ngozi za cilengedwe . Dzifunseni kuti , ‘ Kodi ndakhala ndikumvela Yehova kwa nthawi yaitali bwanji ? ’ 2 : 10 ) Koma kodi angacite bwanji zimenezi ngati samvetsetsa cinenelo cimene cikambidwa mumpingo mwawo ? Yesu anatonthoza anthu mwa kuwapatsa malangizo anzelu , kucita nawo zinthu mokoma mtima , ndipo nthawi zina anali kucilitsa odwala awo . Yehova amafuna kuti tiziganizila abale ndi alongo athu amenewa ndiponso ubwenzi wao ndi iye . 10 KUONA ZOLAKWA MOYENELELA Kodi ulosi umenewu unakwanilitsika ? Pa nthawi inanso , Yesu ali ndi zaka 12 , Mariya anali kumvetsela pamene Yesu anali kukamba zinthu zodabwitsa . Paulo analemba kuti : “ Anthu inu musamakhale ndi ngongole iliyonse kwa munthu aliyense , kusiyapo kukondana , popeza amene amakonda munthu mnzake wakwanilitsa cilamulo . Kumva cisoni na kuvutika maganizo Pamene ticita phunzilo laumwini , timakhala tikumvetsela kwa Yehova , koma timakamba naye mwa kupemphela . Iye anauza Pilato kuti cimene anabwelela pa dziko lapansi ni “ kudzacitila umboni coonadi . ” — Ŵelengani Yohane 18 : 37 . ( Agal . 2 : 5 ) Kukonda Mulungu kumatilimbikitsa kuuzako ena za Ufumu wa Mwana wake , amene ‘ adzakwela pahachi yake cifukwa ca coonadi ” pa Aramagedo . ( Sal . 45 : 4 ; Chiv . Komabe , Yesu sadzakhala yekha pothandiza anthu kuti akhale angwilo . Iye anapangadi cosankha , koma kodi mumamvela bwanji mukaganizila cosankha cimene anapanga ? Mtumwi Paulo anapewa khalidwe limeneli , ndipo anapeleka citsanzo cabwino pankhani yoonetsa cikondi ceni - ceni poyamikila ena . Komabe , titakhala zaka zitatu na hafu mu Africa , tinabwelela ku America kuti tikayambe udindo wolela ana athu . Koma kodi pemphelo lingakuthandizeni bwanji kucepetsako nkhawa ? — Sal . 94 : 18 , 19 . 24 : 14 ; Luka 10 : 27 ) Timayendanso m’cikondi mwa kukhala oleza mtima , okoma mtima , ndi okhululuka . N’zinthu ziti zimene zingapangitse kuti muzicita manyazi poimba ? mmene timapindulila ndi misonkhano yampingo . Cifukwa cina n’cakuti Yehova amadziŵa bwino zimene tingakwanitse kucita . Asa anadalila Yehova pamene asilikali a ku Itiyopiya 1,000,000 anabwela kudzamenyana ndi dziko la Yuda . Koma iye analephela kudalila Mulungu pamene Basa anayamba kumanga mpanda wolimba kuzungulila mzinda wa Rama , umene unali m’malile mwa dziko la Yuda . Ndithudi , akulu akatiwongolela mwacikondi ndi mokoma mtima pamene tayamba kuloŵela “ njila yolakwika ” mwina mosazindikila , zimaonetsa cikondi ca Yehova pa ise . — Agal . Koma ngati taugwilitsila nchito molakwika , ungatenthe nyumba ndi kupha anthu . Baibulo limalonjeza kuti Yehova adzadalitsa onse amene amasinkhasinkha Mau ake , ndi kuyesetsa kucita zimene aphunzila . CA M’MA 1910 , makolo anga anasamukila ku Canada kucoka ku Tbilisi , m’dziko la Georgia , ndipo anakakhala m’nyumba inayake yaing’ono pa famu ya kufupi na kumudzi wa Pelly , m’cigawo ca Saskatchewan ku western Canada . “ Ndinali ndi mafunso ambili okhudza moyo , koma abusa a ku Chalichi sanandiuze mayankho ogwila mtima . Akristu amenewa asanasankhidwe ndi Yehova kuti adzapita kumwamba , anali ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha padziko lapansi . ( b ) Nanga n’ciani cikucitika masiku ano cimene cingafune kuti tikhale maso ? ( Yohane 17 : 11 ) Tikamatsatila mfundo za m’Baibulo pa umoyo wathu ndi kugwila nchito yolalikila , timadziŵa bwino makhalidwe a Mulungu apamwamba . Komabe , kuti tikhale na ufulu umenewu na kupindula nawo , tifunika ‘ kutembenukila kwa Yehova , ’ kutanthauza kukhala naye paubwenzi wabwino . Kodi citsanzo ca Petulo cimatilimbikitsa bwanji ? Kodi iye anasintha maganizo ake pamene ansembe anamucenjeza za khalidwe lake lodzikuza ? Mwacitsanzo , Nowa ndi banja lake anamanga cingalawa . Koma makolo ake anamuphunzitsa za Yehova ndi colinga cake cakuti adzaombola Aheberi ku ukapolo ndi kuwapatsa Dziko Lolonjezedwa . ( Gen . 7,876,000 Tingapeze mapindu abwanji ngati tilemekeza anthu amene ayenela kupatsidwa ulemu ? ( b ) Kodi ana angacite ciani kuti apindule ndi zaka zao zaunyamata ? ( Machitidwe 28 : 8 ) Koma Paulo sanacilitse aliyense amene iye anali kudziŵa . Iye analonjeza kuti adzacotsapo kupanda cilungamo ndi kudalitsa atumiki ake okhulupilika mwa kuwapatsa moyo wosatha m’dziko latsopano la cilungamo . — Ŵelengani Salimo 37 : 5 , 7 , 9 , 29 . MTENDELE Tidzakambilana za Yakobo , Mariya , na Yesu . Ndipo olo kuti tinabatizika , pali zinthu zina zimene timafunika kuwongolela . Cikumbutso ca Imfa ya Khristu cidzacitika pa Ciwelu , pa March 31 , 2018 . Usiku wakuti maŵa aphedwa , Yesu anauza otsatila ake kuti azikumbukila imfa yake mwa kucita mwambo wosavuta . Jan wa ku Sweden wa zaka 66 anati : “ Ukamakonda ena , ionso amayamba kukukonda kwambili . ” Patapita miyezi itatu , Alexandra anakondwela kwambili kuonananso ndi mnyamata wacichainizi ameneyo pa msonkhano wa cigawo wa Mboni za Yehova wa cinenelo ca Cichainizi ku Peru . 20 : 13 , 26 - 30 ) Koma Asa , anadalila Mulungu , ndipo Yehova anayankha pemphelo lake . 11 , 12 . ( a ) N’ciani cimene acicepele angacite kuti akonzekele bwino ulaliki ? Baibo imakamba za mphatso yamtengo wapatali m’mau odziŵika bwino akuti : “ Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha , kuti aliyense wokhulupilila iye asawonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” — Yohane 3 : 16 . Ndinali kuseŵenza kuyambila 23 : 00hrs mpaka 07 : 00hrs . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Thetsa nkhani mofulumila . ” — Mateyu 5 : 25 . Ndinali kukhumbila ana ena amene anali ndi atate ao . Abale amene akukalamila ayenela kukumbukila ciyeneletso cina ca akulu , cakuti ayenela ‘ kukhala zitsanzo kwa gulu la nkhosa . ’ ( 1 Pet . 14 : 10 - 12 ) Kodi zimenezi zinayenela kukhala zodabwitsa kwa Aisiraeli ? Kodi tiphunzilapo ciani tikaganizila mmene Yehova anaonetsela kuti anali kum’dziŵa Mwana wake na mmene anamudalitsila ? Yesu anakamba kuti angelo a ophunzila ake amaona nkhope ya Mulungu . Sitidzacita mantha , koma tidzakhala ndi cikhulupililo cakuti tipulumuka ( Onani ndime 12 ndi 13 ) Ngati zakhala conco , muyenela kumvela Yehova ndi kucita zinthu mokoma mtima kwa Mkristuyo monga mmene Natani anacitila . Nthawi zina , ngakhale anthu amene atumikila Yehova kwa nthawi yaitali amamva manyazi , ndipo zimakhala zovuta kuti aphunzitse ena . Mwacitsanzo , Adamu na Hava atapandukila Mulungu , anakhala na ufulu wodziikila okha miyezo ya cabwino na coipa . Nazonso ziŵanda zinakhala na mphamvu yolamulila maboma a anthu . ( Gen . Tikamacita zimenezi , ndiye kuti tidzalandila madalitso amene Yehova adzapeleka pa nthawi ya kukwanilitsidwa kwa lonjezo lakuti : “ Cilengedweco cidzamasulidwa ku ukapolo wa kuvunda n’kukhala ndi ufulu waulemelelo wa ana a Mulungu . ” — Aroma 8 : 21 . Zaka 2 sauzande kucokela pamene Yehova anapeleka ciweluzo kwa Satana , iye analamula kholo lakale Abulahamu kuti acoke mumzinda wa Uri wa ku Mesopotamiya , ndi kupita kudziko la Kanani . ( Mac . ( 1 Pet . 5 : 13 ) Kukhala ku dziko lina kungakhale kovuta , koma Petulo sanalole ukalamba kumulepheletsa kupeza cimwemwe cifukwa cotumikila Yehova mokwanila . Riana akamba nkhani m’citundu ca Citandiroyi Ndi lamulo lacikondi ndiponso lofunika liti limene Yehova anapatsa Adamu ? Bungwe lina limene limathandiza olemala linandiphunzitsa kusoka zovala . Koma nthawi zina zimenezi n’zosatheka . Anthu ambili othaŵa kwawo amasiya acibale , mabwenzi , ndi mipingo yawo . Mlongo wina wa zaka 18 , amene anabatizika ali na zaka 13 , anavomeleza mfundo imeneyi . Iye anati : “ Zikhulupililo zanga nimazidziŵa bwino , koma nthawi zina nimakangiwa kuzifotokoza . ” Alendowo atadya cakudya cokoma cimeneci anakhalanso ndi mphamvu ndipo anapitiliza ulendo wao . Nili na mkazi wabwino , Elke , mkazi wacikondi ndiponso wacifundo . N’takana , mkulu wa asilikali analamula kuti nitumizidwe ku cisumbu coopsa cimene anali kulangilako akaidi , cochedwa Makrónisos ( Makronisi ) . Kodi Baibulo limati ciani pankhani yokhulupilila Yehova ? 3 : 1 - 5 , 13 ) Kodi mwaona kukwanilitsidwa kwa mau amenewa ? Kuti tipeze mayankho , tiyeni tikambilane zocitika zitatu zimene zingatiike paciyeso pa nkhani ya kudzicepetsa . Tidzaonanso mmene tingacitile mwanzelu pacocitika ciliconse . — Miy . Iwo amayesetsa kusamalila odwalawo cifukwa amafuna kuwathandiza . Kodi zimene Abele anali kuganiza ponena za mtsogolo zinali zozikidwa pa ciani ? MU 1871 , moto unabuka m’nkhalango ya Wisconsin , ku United States . Poona kuti ziphunzitso za chechi zinali zosagwilizana ndi malemba , iwo anayamba kuzikana . Koma amene anali kulankhula zimenezi poyela , anali kupatsidwa cilango coopsa , ngakhale kuphedwa kumene . Kodi mufuna kulimbitsa cikhulupililo canu m’malonjezo a Mulungu a mtsogolo ? 6 Mudzacitapo Ciani pa Mphatso ya Mulungu Yopambana Zonse ? ( Ŵelengani Salimo 133 : 1 , 2 . ) Munacita ndendende zimene Baibulo limatilimbikitsa kucita : Kupitiliza ‘ kufufuza ’ kuti timvetsetse . Kodi mungatengele bwanji citsanzo ca Asa potumikila Yehova ? Masiku ano , Baibo siipezeka cabe monga buku lopulintiwa , koma imapezekanso pa kompyuta . Kodi Yehova amaseŵenzetsa bwanji zinthu zake mooloŵa manja ? M’masiku amenewo , ni mmene zinthu zinalili m’madela ena . Akamamvetsela mapemphelowo , Yehova amakambanso ndi angelo ndi kuwapatsa malangizo . Ngakhale kuti Yehova ndi Mulungu wacikondi , kodi amadana ndi ciani ? Mabanja ambili akupindula cifukwa cotsatila malangizo a m’Baibulo . M’nthawi ya Yesu , mneneli wamkazi Anna atakhala m’cikwati zaka 7 cabe , mwamuna wake anamwalila . M’bale Yury anati : “ Nthawi zambili tinali kupemphela kwa Yehova kuti atithandize kukhala olimba ndi kuti tipitileze kumudalila pogwila nchito yolalikila . N’ciani cidzacitika ukwati wa Mwanawankhosa ukalibe kucitika kumwamba ? Muziyesetsa kuwathandiza pa zosoŵa zawo , m’malo moganizila kwambili za kayendetsedwe ka zinthu mu mpingo . ” 18 : 11 ) Yesu ananena fanizo losonyeza zimene zimacitikila “ munthu amene wadziunjikila yekha cuma , koma amene sali wolemela kwa Mulungu . ” Mu July 2007 , Katherine ali ndi zaka 26 anasamukila ku Saipan , kacilumba ka pa Nyanja ya Pacific , mtunda wa makilomita 10,000 kucokela kwao . Phili la Tabori ndi lalikulu koma lafulati pamwamba pake . ( Yakobo 4 : 8 ) Nthawi zina , tikhoza kukaikila ngati n’zothekadi kukhala pa ubwenzi na Mlengi wamphamvu yonse . 20 : 3 . Kodi Yehova anayankha bwanji mapemphelo ao ? Mtumiki ameneyo atamuneneza kuti anali kusakaza cuma ca bwana wake , “ anacita mwanzelu ” mwa ‘ kudzipezela mabwenzi ’ kuti adzam’thandize akadzacotsedwa nchito . Mwacitsanzo , m’bale wina anapita kukacita ulendo wobwelelako kwa munthu wina wacikulile amene wakhala akuŵelenga magazini athu kwa zaka zambili . Pangani zosankha zimene zidzakuthandizani kutumikila Yehova mosangalala m’nthawi yapadela ino . — Sal . Mlingo wa nchito yolalikila ndi kufalikila kwa nchito yolalikila uthenga wabwino padziko lonse ku mitundu yonse ya anthu . Mau akewo aonetsa kuti Mariya anali kudziŵa bwino Malemba Aciheberi . Muziyesetsa kuseŵenzetsa zimene mwaphunzila Ndiponso ngati tiyang’anitsa galasi kwina , tingaone cithunzi ca munthu wina . Iye ndi amene anatipatsa moyo . N’tafika zaka 11 , n’nayamba kumwa mowa . Yesaya anadabwa nazo zimenezi ndipo anafuna kudziŵa kuti mtundu wosankhidwa wa Mulungu udzakhalabe wosalapa kwautali wotani . Ngati tiseŵenzetsa Mau a Mulungu pophunzitsa , tingathandize mwana wathu kapena wophunzila Baibo kumvetsetsa na ‘ kusunga zinthu zonse zimene Yesu anatilamulila . ’ ( 2 Tim . 3 : 16 ; Mat . KODI munalionapo dzina la Yehova litalembedwa pa zipupa za nyumba kapena pa zinthu m’nyumba zosungilamo zinthu zakale ? Mungamuuze kuti lesipi ya apozi imeneyi “ inalembedwa ” mkati mwa kambewu aka , koma m’malangizo amene ife anthu sitingamvetsetse . ( Machitidwe 1 : 8 ) Kenako , anthu ambili anayamba kusonkhana pamene panali Akristuwo , ndipo ophunzila a Yesu anayamba kulankhula zinthu zodabwitsa zimene anamva ndi kuziona . Zimene zinacitikila Yobu zitiphunzitsanso kuti tifunika kuonetsa cifundo kwa Akhristu anzathu amene akukumana na mavuto . 31 : 8 . Kodi makolo a Blossom anali kufuna kutsimikizila ciani ? Kodi Yehova anamuuza ciani ? MGWILIZANO WA ANTHU AMITUNDU YOSIYANA - SIYANA Ndiponso , cifukwa copita mu utumiki kaŵilikaŵili , ndinayamba kuikonda kwambili nchitoyi , cakuti ndinayamba kulakalaka kukhala mpainiya . Koma anzangawo anafuula kuti “ Iyai kucita zimenezo n’kulakwa ! Tate wina anati : “ Osatenga mafunso a mwana wanu mopepuka . Panthawi imeneyo , m’dziko la Isiraeli munabwela gulu la acifwamba . 5 ( b ) Ni lumbilo lanji limene Mfumu Zedekiya analephela kusunga ? Mkwati , amenenso ndi Mfumu , adzayamba kulamulila dziko lapansi ndi kuukitsa ‘ makolo ake ’ amene adzakhala “ ana ” ake a padziko lapansi . ( Yoh . 5 : 25 - 29 ; Aheb . N’cifukwa ciani n’kofunika kuti anthu tsopano akhale okhulupilika kwa “ Mfumu ” ndi “ abale ” ake ? 1 : 15 . Yesu anati : “ Cumaco cikatha , ” osati ‘ ngati cumaco catha , ’ kusonyeza kuti cuma cakuthupi n’cosadalilika , cidzatha . Kukamba kwina , osalungama akamwalila ndiye kuti alipila macimo ao . Cifukwa cacitatu n’cakuti kukhala na zolinga zauzimu mukali aang’ono kumathandiza popanga zosankha . Ophunzila Baibo anali okangalika pa ulaliki ! Akazembe saloŵelela m’zocitika za m’dziko limene atumidwa kukatumikilako . 9 : 6 , 7 , 56 : 10 ; Dan . 2 : 44 ) Conco ngati tikhala maso mwauzimu , tidzakhala okonzekela tsiku la ciweluzo . — Sal . Iye anati : “ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ” Tiyeni tikambilane atatu a mavuto amenewo , ndi kuona mmene ena amene anasamukila ku Micronesia anawagonjetsela . Nthawi ina iliyonse , mtumiki wa Yehova angakumane ndi ciyeso , ndipo angafunike kucita zinthu mosiyana ndi anzake a kunchito , a kusukulu , acibanja , ndi ena . ( 1 Pet . Iwo anali atsogoleli acipembedzo Aciyuda amene anacititsa kuti Yesu aphedwe . Cakumapeto kwa zaka za m’ma 1800 , Charles Taze Russell ndi anzake ena anayesetsa kukhazikitsanso kulambila koona kwa Cikhiristu . Popeza mnyamatayo analibe ndalama , Alexandra anamubweleka ndalama zokwana madola 20 . Mose atafa , Yoswa , amene anamuloŵa m’malo , analimbikitsidwa ndi “ kalonga wa gulu lankhondo la Yehova ” kuti atsogolele anthu a Mulungu kukamenyana ndi Akanani . Aisiraeli anapambana nkhondoyo . ( Yos . Monga mmene zizindikilo zosiyana - siyana zimathandizila dokota kudziŵa matenda a wodwala , zizindikilo zochulidwa m’maulosi amenewo zinan’thandiza kudziŵa kuti tikukhaladi mu “ masiku otsiliza ” ochulidwa m’Baibo . Ŵelengani Yohane 15 : 9 , 10 . Julia , wa zaka 16 , anati : “ Nimakhala na zofalitsa m’cola canga ca ku sukulu . Komanso , nimayesetsa kumvetsela zimene anzanga amakamba kuti nidziŵe maganizo awo na zikhulupililo zawo . Sukuluyi ikucitikabe m’madela ena ambili , ndipo abale ophunzitsidwa bwino ndi amene amatumikila monga alangizi . Mwacitsanzo , Mulungu anateteza abale athu panthawi ya ulamulilo wa Nazi ku Germany ndi m’maiko ena m’zaka za m’ma 1930 mpaka kumayambililo kwa 1940 . Mwacitsanzo , ndikumbukila bwino tsiku limene ndinapita kunyumba kwao pamene tinali pa cibwenzi . Iwo ali ndi udindo wofunika kwambili . Nkhondo : Nkhondo ziŵili za pa dziko lonse zimene zinacitika , zinapha anthu pafupi - fupi 60 miliyoni kapena kuposelapo . ( Mateyu 18 : 20 ) Baibulo limakambanso kuti Yesu ‘ amayenda pakati ’ pa mipingo . Tiyeni tikambilane zitsanzo zitatu za mmene tingacitile zimenezi . Baibulo — Kodi Ndilo Mawu a Mulungu Kapena a Munthu ? — Buku limeneli n’laling’ono koma lili na mfundo zimene zinafufuzidwa mosamala , ndipo limafotokoza umboni woonetsa kuti Baibo ni Mau a Mulungu ouzilidwa Pamene mwabatizidwa , mumaonetsa ena kuti munadzipeleka kwa Yehova . ( Ŵelengani Miyambo 11 : 2 . ) Inu pamwekha , mungacite ciani kuti mutonthoze ena ? Kudzicepetsa kudzatithandiza kukhala ogonjela kwa anthu amene akutitsogolela . Ndipo kukhala ogonjela n’kofunika kwambili kuti mu mpingo mukhale mgwilizano . Kumeneko , n’nali na mnzanga watsopano wocita naye upainiya , koma kunalibenso mpingo . Komabe , zimakhala zosavuta kukhumudwa cifukwa ca matenda , kusoŵa ndalama , kapena cifukwa cakuti sitikupeza anthu acidwi mu ulaliki . Mkwatibwi ameneyu amachedwa “ mwana wamkazi ” komanso “ mwana wamkazi wa mfumu . ” ( Sal . ( Mateyu 19 : 11 , 12 ) Anthu amene sali m’cikwati ali ndi maudindo ocepa kuposa anthu a m’cikwati . Mau a Mulungu angakuthandizeninso kudziŵa ngati cikhulupililo canu n’colimbadi . — Ŵelengani Yakobo 1 : 25 ; 2 : 24 , 26 . Koma mu 1990 anayamba kusintha maganizo ake . Pamene Yosefe anali na zaka pafupi - fupi 20 , abale ake anamugwila ndi kum’gulitsa monga kapolo . 29 : 31 - 35 ; 30 : 22 - 25 ; 35 : 22 - 26 ; 49 : 22 - 26 ; 1 Mbiri 5 : 1 , 2 ) Ngakhale n’conco , mzela wa makolo a Mesiya sunapitile mwa Rubeni kapena Yosefe , koma mwa Yuda , mwana wacinayi wa Yakobo kwa Leya . — Gen . Koma kwa munthu sizikhala conco . Tikaona mmene alonda akale anali kulondela mizinda , tingaphunzilepo cinthu cimodzi . Cotsilizila , m’malo moyesa kuthetsa tekha vuto , tifunika kuyesetsa kukhalabe okhulupilika ndi kuyembekezela Yehova moleza mtima kuti ndi amene adzathetsa vutolo . Monga makolo acikhristu , mungamulimbikitse kuti akaonane na akulu kuti akam’pende ngati ali woyenelela kubatizika . Iwo adzaulukila m’mwamba ngati ali ndi mapiko a ciwombankhanga . ” Nditamaliza sukulu , ndinayamba nchito yaganyu yophunzitsa Cingelezi n’colinga cakuti ndicite upainiya . Koma adzalandila cidindo comaliza akalibe kufa kapena cisautso cacikulu cisanayambe . — Chivumbulutso 7 : 1 , 3 . Cikondi n’cimene cimatilimbikitsa kupilila . Pangano limeneli limachedwa pangano la Ufumu . ( Pitani pa BIBLE TEACHINGS > BIBLE QUESTIONS ANSWERED > FAMILY ) Ngati makolo anu ali ndi matenda osacilitsika , mungafunikile kusintha njila zoŵasamalila kapena kusintha zinthu zina m’nyumba yao . N’cifukwa ciani m’pofunika kusamala ndi anthu ogwilizana nao masiku ano otsiliza ? Njila imodzi imene amacitila izi ni mwa kutipatsa ciyembekezo cakuti posacedwa adzathetsa zoipa zonse padzikoli . Yobu anati : “ Kodi amene anandipanga m’mimba si amene anapanganso iyeyo ? ” “ KODI WAONA MMENE AHABU WADZICEPETSELA ? ” Yesu anakamba kuti Yehova amapeleka “ mzimu woyela kwa amene akum’pempha . ” Ili ni cenjezo lamphamvu kwa anthu amene amakonda zosangalatsa mopambanitsa . ( Sal . 37 : 18 ) Inde , iye amaona mavuto amene timakumana nawo , ndipo angatipatse mphamvu zotithandiza kupilila vuto lililonse . Malinga n’zimene anthu amenewo anakamba , kuphatikizapo ena mamiliyoni ambili , kuŵelenga Baibo kungakuthandizeni kukhala na umoyo wacimwemwe . Ndife okondwa kwambili kuti posacedwapa Yehova adzaononga imfa , mdani wotsilizila . Tinayenda pa sitima kwa makilomita 6,000 , n’kukafika mumzinda wa Tulun , ku Siberia . Betuele ndi Labani anakondwela kwambili ndi nkhani ya Eliezere . ( Genesis 30 : ​ 32 , 33 ; 31 : ​ 38 - ​ 40 ) Mitundu iŵiliyi ya ziweto inali kutsekeledwa m’makola osiyana ndi colinga cakuti ateteze nkhosa zofatsa , zazikazi , ndi zimene zili ndi tuŵana , kuti zisapwetekedwe ndi mbuzi zazikali . Conco , Jairo anabatizidwa ndi kukhala wa Mboni za Yehova ali ndi zaka 17 . Conco , nayenso analoŵelelapo . ( Afil . 2 : 5 - 11 ) Ifenso tikhoza kudalitsidwa ngati timakhulupilila Yehova ndi mtima wonse . PACISANU m’maŵa , mu September 1922 , anthu okwana 8,000 anakhamukila m’ciholo cacikulu . Panthawiyo kunja kunali kutayamba kale kutentha . 1 : 8 ) Nawonso mafumu amene analamulila anthu a Mulungu anatsatila zimenezi . Amacititsanso munthu kukunyuka , kulephela kudya , ndi kuvutika kulankhula . Baibulo limati : “ Debora nayenso anapita nao . ” Patapita nthawi yocepa , Daniel anamwalila . Ngati siconco , kodi sicingakhale bwino kuvomeleza zimene waniuza ? ’ Ganizilani zimene mukumana nazo , zimene zingakhale ciyeso kwa inu . Nthawi inayake pambuyo pa Cigumula , Nimurodi anayamba kucita zinthu motsutsana ndi Yehova , koma Nowa anapitilizabe kukhala ndi cikhulupililo ndiponso ciyembekezo . ( Gen . Ngakhale n’conco , sitisoŵa cakudya ndipo ‘ dzanja la Yehova si lalifupi . ’ Tikadzamvela malangizo ‘ olembedwa m’mipukutuyo ’ ndi kukhalabe okhulupilika kwa Yehova pa ciyeso comaliza , iye adzalemba maina athu mu “ mpukutu wa moyo . ” “ Panthawi ya cakudya ca m’madzulo , aliyense wa ise amafotokoza cinthu cimodzi cokondweletsa ndi cina cosakondweletsa cimene cacitika pa tsikulo . Ndi iko komwe , timapemphedwa ‘ kuyenda modzicepetsa ndi Mulungu wathu . ’ Mothandizidwa ndi Mau a Mulungu ndiponso mzimu wake woyela , timayesetsa ‘ kuvula umunthu wakale ’ na ‘ kuvala umunthu watsopano . ’ — Akol . ( Sal . 24 : 3 , 4 ) Kodi Hana ndi Yefita analonjeza ciani ? Nanga kodi cinali copepuka kwa iwo kukwanilitsa malonjezo awo ? Yesu anatiphunzitsa kuti sitiyenela kudela nkhawa za cakudya ndi zovala , koma tiyenela kupitiliza kufunafuna Ufumu coyamba . Pampingo wina analipo yekha mkulu ndipo anali kusamalila ofalitsa oposa 100 . Mulungu amene anali kulambila anali ataonekela kwa iye na kukamba naye , mosakaikila kupitila mwa mngelo . Kodi mau akuti “ copondapo mapazi ” amaimila ciani m’Malemba Aciheberi ? ( Aroma 1 : 7 ) Conco , Paulo anali kusiyanitsa Akhiristu oyenda motsatila za thupi ndi Akhiristu amene anali kuyenda motsatila mzimu . Anthu amene sakonda Yehova angayese kukusonkhezelani kuti mukhale ndi mzimu wokonda dziko . Anamuuzanso kutenga cakudya ndi madzi okwanila mofanana ndi anchito ake . Mkazi wake Kendra , anam’limbikitsa kuti avomele ciitano cimeneco . Pa vesi 10 ndi 13 , Yehova analonjeza kuti : “ Usacite mantha , pakuti ndili nawe . Ngati mungakonde , ŵelengani mavesi amenewa . Zoonadi , n’zotheka kuti mwamuna ndi mkazi azisangalala m’banja ndi kuthandizana panthawi zovuta . — Miy . Wosimba ndi Stephen Mcdowell Koma kodi iwo angapambane pa nkhondo yolimbana na angelo oipa ? Tikambilana zimenezi m’nkhani ziŵilizi , ndipo tiphunzilanso mmene Baibulo la Dziko Latsopano lathandizila anthu kulemekeza dzina la Mulungu ndi kudziŵa cifunilo cake . Ngakhale n’conco , atumikiwo anayesetsa kumvela Cilamulo ca Mulungu . Baibulo limati : “ Mulungu wakumwamba adzakhazikitsa ufumu [ boma ] umene sudzawonongedwa ku nthawi zonse . ( Maliro 2 : 17 ; Ezek . 5 : 11 ) Nthawi ikubwela pamene iye adzawononga onse amene safuna kumumvela . Conco ndinapemphela kuti ndipambane . M’mbili yonse ya anthu , adani akhala akuononga Baibulo komanso kupha anthu omasulila ndi kufalitsa Baibulo . Tikapitiliza kuphunzitsa cikumbumtima cathu , timayamba kuona zinthu monga mmene Yehova amazionela . Coyamba tingavomelezane naye kuti anthu oipa adzalandila cilango . Yankho ni INDE ! Pamene Mfumu Koresi anamasula Aisiraeli mu ukapolo , kodi iwo ayenela kuti anamvela bwanji ? ( Ŵelengani Luka 11 : 10 - 13 . ) Akulu anzanga ndiponso woyang’anila wadela ananithandiza kwambili kuona zinthu moyenela . Katswili wa Baibulo dzina lake Richard Elliott Friedman anakamba kuti : “ Mfundo yaikulu inali yakuti cilango cimene cinali kupelekedwa cinali kufunika kukhala cofanana ndi mlandu umene munthu wacita . ” Pofika pano , iye anali kudziŵika kuti Abulamu . “ ‘ Bwenzi lathu Lazaro ali m’tulo akupumula , koma ndikupita kumeneko kukamudzutsa ku tulo take . ’ Mu Baibulo la Dziko Latsopano losakonzedwanso , liu lakuti Asher linamasulidwa kuti “ iwo ” [ “ anthuwo ” ] . Ndikhulupilila kuti takambilana zinthu zambili zatsopano zofunika kuziganizila . Yehova anacha Abulahamu , kholo la Aisiraeli kuti ‘ bwenzi lake . ’ ( Yes . Molingana na zimenezi , ambili a ise timakhala ndi kuseŵenza pamodzi na anthu a makhalidwe osagwilizana ndi a Mulungu . Mofananamo , Malaki caputala 3 amachula za kuyendela kacisi wa kuuzimu , ndiyeno pambuyo pake kuuyeletsa . ( Mal . Ndiphunzitseni zoonjezeleka zokhudza Baibulo . ” Amene akukila mu mpingo mwanu : Akhristu ena angakukile m’dela lanu . Mulungu adzacotsa ucimo ndi imfa zimene tinatengela kwa Adamu . Tikavala umunthu watsopano , timayamba kutengela makhalidwe a Yehova . ( Akol . Monga mmene zinalili ndi Isiraeli wakuthupi , Isiraeli wa kuuzimu ndi anthu amene Yehova anakamba kuti “ anthu amene ndinawapanga kuti akhale anga , anene za ulemelelo wanga . ” MFUNDO YA M’BAIBO : “ Musamakwiyitse ana anu , kuti angakhale okhumudwa . ” — Akolose 3 : 21 . Koma zimenezi n’zosiyana kwambili ndi zimene Baibulo limanena . Kodi mukumbukila mabodza amene nthumwi ya Asuri , Rabisake , anaseŵenzetsa polimbana ndi anthu a Mulungu ? Atacoka m’cipatala , Kumiko anapita kukaonako ku dziko la Nepal . Pambuyo pake iye ndi mpainiya mnzake anakukila ku Nepal . Ndili ndi zaka 7 , ndinagwilizana ndi bungwe la anyamata lochedwa Boy Scouts . Munthu wa m’fanizo limeneli amaimila mlaliki wa Ufumu aliyense . 1 : 10 ) Komabe , mofanana ndi dalaivala uja amene amalephela kusamalila injini ya galimoto yake , akulu ambili amatangwanika kwambili kusamalila maudindo ena cakuti amanyalanyaza kuphunzitsa ena . Pamene muphunzila , simuyenela kukhala na colinga cowonjezela cabe cidziŵitso . Conco , cikondi ndi cifundo cake , zinamusonkhezela kuombola anthu mwakucita cinthu cacikulu . Cinthu cimeneci cinali kupeleka Mwana wake kuti atiombole . — Aroma 5 : 6 - 8 Ngati iye anyalanyazabe kusintha oilo mu injini , tsiku lina galimotoyo ingaonongeke kwambili ndi kulekelatu kuyenda . Kumasuka mu Ukapolo , Na . Imafotokoza kuti : “ Iye amene ali Mfumu ya olamulila monga mafumu ndi Mbuye wa olamulila monga ambuye , . . . Iye yekha ndiye amene ali ndi moyo wosakhoza kufa , amene amakhala m’kuwala kosafikilika . Mwaona ka , pafunika aphunzitsi a Baibulo ambili cakuti ngakhale ophunzila Baibulo acita kukhala aphunzitsi a Baibulo . Monga mmene Mulungu amakhalila woleza mtima ndi wokoma mtima kwa anthu opanda ungwilo , ifenso tiyenela kukhala oleza mtima ndi okoma mtima ngati ena atilakwila ndiponso ngati alankhula mosaganizila kapena mwamwano . Yesu nayenso ali ndi mphamvu yocilitsa odwala . Kodi a m’cikwati afunika kuonetsa mitundu iti ya cikondi ? Yesu anali na nthawi yocepa yolalikila . Timatha kuyelekezela m’maganizo mwathu zimene zidzacitika mtsogolo . Komabe , aliyense wa ife angakondweletse Yehova ndi kupeza cipulumutso ngati tipitilizabe kumutumikila mokhulupilika . — Mat . Ndani anakhala mtundu watsopano wa anthu a Yehova m’nthawi ya atumwi ? ( Yes . 65 : 16 ) Ngati ticita khama kulimbana na zopinga n’colinga cakuti tiwonjezele utumiki wathu , tidzalandila madalitso ocokela kwa Yehova . Conco , tifunika kuonana ndi abale othaŵa kwawo mwamsanga akangofika m’dela lathu . Nanga ndani ayenela kulalikila ? Mukatelo , mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu . ” — Afilipi 4 : 6 , 7 . Pokhala Mfumu ndi Mkulu wa Ansembe , Yesu ndiye mtsogoleli wa gulu lankhondo lakumwamba la Yehova . ( Sal . 76 : 11 ) Pa malonjezo onse amene timapanga , lonjezo lofunika kwambili ndi la kudzipeleka kwathu kwa Yehova . Koma cimene tiyenela kukumbukila n’cakuti , Yesu anali kumvela cifundo odwala ngakhale kuti iye sanadwalepo . 12 : 9 ; Gen . Mwina tingadzifunse kuti , “ Kodi ndili ngati Msamariya kapena ndili ngati wansembe ndi Mlevi ? Mwa zocita zathu zabwino , timaonetsa kuwala kwathu ndi kucititsa kuti dzina la Yehova lilemekezeke . Ambili pogwila nchitoyi anangosaina kuti cicitike cicitike ! Kuonjezela apo , ubwenzi wanga ndi Yehova walimba kwambili kuposa kale . ” Mabuku onse anayi a Uthenga Wabwino amakamba kuti mtembo wa Yesu atautsitsa pamtengo wozunzikilapo , Yosefe anaukulunga munsalu yabwino kwambili na kukauika m’manda ake . ( Mat . Ngati Akristu amenewo acita chimo lalikulu ndipo sanalape , tifunika kuleka kugwilizana nao . — Aroma 16 : 17 , 18 . 11 , 12 . ( a ) Kodi kudzicepetsa kungatithandize bwanji ngati ena atiyamikila kapena kutitamanda mopambanitsa ? Conco , akalosela amadziŵa bwino mmene anthu adzakwanilitsila maulosi ake . Iwo amatumikila m’mipingo yao kapena kumalo osoŵa . Apainiya apadela amapeleka maola 130 pa mwezi . Hava anakopeka na mfundo yabodza ya Satana yakuti “ maso anu adzatseguka ndithu , ndipo mudzafanana ndi Mulungu . Mudzadziŵa zabwino ndi zoipa . ” ( Gen . 7 : 1 ) Mwacitsanzo , ngati wina wavulala kwambili pa ngozi ya pa mseu ndipo am’peleka mofulumila kucipatala , kodi coyamba a dokotala ndi anesi angafune kudziŵa ngati munthuyo ndiye wacititsa ngoziyo ? Iyai . ( Yuda 20 , 21 ) Nanga bwanji ngati muona kuti zimene mumacita sizicokela pansi pa mtima , koma mumangozicita mwamwambo cabe ? Popeza kuti pansi pa nyanjayo pali mdima , n’kosavuta kuti mphamvu ya dzuŵa ilowe pansi pa nyanja ndipo zimenezi zingapangitse kuti madzi oundanawo apitilize kusungunuka . ( 2 Pet . 3 : 13 ) Koma pali pano , tiyembekezela gulu la Mulungu kupitilizabe kukula . ( Yes . 35 : 5 , 6 ) Ganizilani mmene tidzasangalalile kuceza ndi acibale , anzathu , kuphatikizapo amene adzaukitsidwa . ( Yoh . Ndife oyamikila kuti Yehova sanatiikile malamulo ambili - mbili pa nkhani ya mavalidwe ndi kudzikonza . ( Yobu 6 : 14 ) Komanso , iye sanali kudzikweza pamaso pa ena , koma anali kudela nkhawa anthu onse , kaya olemela kapena osauka . ( Yesaya 2 : 2 , 3 ) Ndife osangalala kwambili kuona ulosi umenewu ukukwanilitsika masiku ano . N’cifukwa ciani munthu aliyense afunika kupatsidwa ulemu ? Ndipo n’naona monga kuti natayika . ” Yesu anadziŵa kuti mavuto a zacuma sadzathelatu m’dzikoli mpaka pamene Ufumu wa Mulungu udzabwela . ( Yohane 4 : 21 ) Mau amenewa ndi odabwitsa kwambili , makamaka cifukwa cakuti amene anawakamba anali Myuda . Koma Yesu sanakambe kuti tiyenela kuonetsa khalidwe limeneli kokha kwa abale ndi alongo athu m’cikhulupililo . Kuti muyankhe funso limeneli , coyamba muyenela kudzifunsa mafunso monga awa : ‘ Ndimamva bwanji kukhala mbali ya mzela wautali wa mboni zokhulupilika ? Sin’nalekeletu kugwila nchito ya udokota . Koma nimaseŵenzetsa nthawi na mphamvu zanga zoculuka pothandiza kucilitsa anthu mwauzimu , ndi kuthandiza abale na alongo mu mpingo . Izi zimanipatsa cimwemwe mumtima ndi kunithandiza kukhala okhutila . ” Komabe , zimene zinacitika pambuyo pake , ziyenela kuti zinayesa kudzicepetsa kwawo ndi kudalila kwawo Yehova . Ambili angakopeke na maganizo a dziko amenewa . Anauza ana awo kuti : “ Ndeke zimaoneka monga mbalame . N’cifukwa ciani tifunika kucita khama mwanjila imeneyi ? Kodi mungalione bwanji dzanja la Yehova pa umoyo wanu ? Pamene anamva kuti Yesu ali ndi mphamvu zocilitsa anthu , “ mumtima mwake anali kunena kuti : ‘ Ndikangogwila malaya ake akunja okhawo , ndicila ndithu . ’ ” ( b ) Kodi zinthu zidzakhala bwanji pambuyo pa Ulamulilo wa Khristu wa Zaka 1,000 ? Koma Yehova anacitapo kanthu mwa kuteteza Sara kuti asaipitsidwe . ( Miyambo 15 : 15 ) N’zoona kuti mukamakalamba , mungayambe kukhumudwa mukaganizila masiku anu aunyamata ndi zinthu zambili zimene munali kucita . Komabe , Naoko analeka kukoka . Cikondi n’cofunika kwambili m’banja . 17 : 24 - 27 ) Ndithudi , anthu angam’pezedi Mulungu . Caka catha , Mboni za Yehova zinathela maola oposa 1.9 biliyoni zikulalikila uthenga wabwino m’maiko 240 , m’zinenelo zoposa 700 . ( Aheb . 4 : 15 ) Nthawi zina zimakhala zovuta kumvetsa mmene anthu odwala matenda aakulu akumvela , makamaka ngati ife sitinakumanepo ndi mavuto otelo . Ngati mumalanga ana anu mosasinthasintha , naonso amakhala otetezeka . M’malomwake , analemba kuti : “ Usapse mtima ndipo pewa kukwiya . ( a ) Kodi ophunzila angatengele bwanji citsanzo ca Elisa masiku ano ? Makolo — Thandizani Ana Anu Kupeza ‘ Nzelu Zowathandiza Kuti Adzapulumuke , ’ Dec . ( b ) Nanga Aroma 12 : 3 imati ciani za munthu wodzicepetsa ? Coyamba anawalangiza kukalalikila kwa Ayuda , ndiyeno pambuyo pake anawauza kukalalikila kwa anthu amitundu ina . Baibulo limatamanda mwamuna amene ndi “ waluso pa nchito yake ” ndiponso mkazi amene “ manja ake amagwila nchito iliyonse mosangalala . ” ( a ) N’cifukwa ciani timapitiliza kugwila nchito yolalikila ? Koma “ alonda ” amenewo amakwanitsa cabe kuteteza dziko lawo ku ziwopsezo zocokela kwa maboma kapena anthu . Mwa ici , m’kanthawi kocepa cabe , malo a ofesi ya nthambi anakula kuŵilikiza katatu . Monga Atate wathu wakumwamba , akutipempha mokoma mtima kuti tizipemphela kwa iye , kungakhale kupanda nzelu kulephela kucita zimenezi . — Ŵelengani Afilipi 4 : 6 . Ukapita ku dziko lina n’colinga cokathandiza anthu kudziŵa Yehova , umaonetsa kuti umadalila Mulungu . Kuti cikumbumtima cathu cizititsogolela bwino , tifunika kuciphunzitsa . Conco , n’zosadabwitsa kuti nthawi zina cimamuvuta kupezeka pa misonkhano ya mpingo . Kodi bungwe lolamulila la m’nthawi ya atumwi linamulimbikitsa bwanji Filipo ? 18 , 19 . ( a ) N’cifukwa ciani tifunika kucita khama kuti tikhalebe ndi cikhulupililo ? Ngakhale ndi mau ocepa amenewa , Baibulo limaonetsa kuti zimenezi n’zoona . Pamene uona kugwilizana bwino kwa malemba , iwenso udzavomeleza kuti n’zoona aneneli a m’Baibulo ndi alembi ake ‘ anatsogoleledwa na mzimu woyela . ’ — 2 Pet . * Ofesi ya nthambi itatiuza malo amene tingapiteko , tinapita kumaloko kuti tikafune nyumba yokhalamo ndi nchito . ” Kuwonjezela pa thandizo la amuna okhulupilika monga Heledai , Tobiya , na Yedaya , Mulungu anakamba kuti anthu enanso ambili “ adzabwela kudzamanga nawo kacisi wa Yehova . ” 12 / 15 N’ciani cinam’limbikitsa Daniel kuti asafooke ? Kuganizila mapemphelo anu ndi njila imodzi imene ingakuthandizeni kuona ngati cosankha canu cofuna kubatizidwa ndi cocokeladi pansi pamtima . Ndi mwai wamtengo wapatali kuti Yehova akukamba nafe m’cinenelo cathu . ” Kucitako mbali yaing’ono m’nchito ya Yehova pa zisumbuzi ni dalitso losakambika . ” ndi maphunzilo otani amene ofalitsa Ufumu akhala akulandila ? Yosefe ? Kuwayamikila kumawathandiza kuti azilandila uphungu mosavuta akalakwitsa . ” — Christine . Baibulo ndico cida cofunika cimene timagwilitsila nchito mu ulaliki . ( Aheb . 6 : 1 ) Pa maziko amenewo , Akhiristu ayenela “ kuwonjezela pa cikhulupililo ” cawo makhalidwe ofunika kuti ‘ apitilize kucita zinthu zimene zingacititse Mulungu kuwakonda . ’ — Ŵelengani 2 Petulo 1 : 5 - 7 ; Yuda 20 , 21 . Iye anati : “ Ndikuona kuti Yehova amandikonda kwambili , n’cifukwa cake anandipatsa malangizo mobwelezabweleza . ” Pamene tikula , tingayambe kuyamikila cilango pozindikila kuti timalangizidwa cifukwa ca cikondi . Mwacitsanzo , bungwe lina loona pa zakapewedwe ka matenda lochedwa , U.S . Mlongo wina wa mumpingo mwao anamvela cifundo amai a mnyamatayo ndipo anawauza kuti : “ N’zomvetsa cisoni kuti mwalephela kuphunzitsa mwana wanu . ” M’malomwake , anaonetsa kuti anali bwenzi la Yehova . Nthawi zambili pamakhala cinacake cimene cikumucititsa kuti asamakondenso zinthu zauzimu . ” Yehova anaonetsa kuti ndi Mfumu ya Cilengedwe Conse , ndipo monga Tate wacikondi , anagwilitsila nchito mphamvu zake kuteteza anthu ake . — Ŵelengani Ekisodo 14 : 13 , 14 . YEHOVA ANAKHALA MFUMU YA AISIRAELI N’ciani cimene tiphunzilapo pamenepa ? Zitatelo , Yaeli anatenga cikhomo ndi nsando zimene akazi okhala m’mahema anali kudziŵa kuziseŵenzetsa mwaluso . Kuti tionenso bwino pagona nzelu yosalumphila malile amene Yehova anaika pa ufulu wathu , tiyeni tioneko zitsanzo zina za m’Baibo . Khalani waubwenzi Koma kodi wokana Kristu ndani ? Nanga mau amenewa akutikhudza bwanji masiku ano ? Goliyati anangopitilila ndi masentimita 15 cabe kuposa munthu wamtali kwambili amene anadziŵikapo masiku ano . M’malo mwake , kumatanthauza kukhala paubwenzi wolimba ndi iye . 2 : 21 ; 4 : 1 . Ndi nthawi iti pamene amakhala okonzeka kumvetsela ? Izi zidzacitika ikadzatha mbali yoyamba ya cisautso cacikulu , koma nkhondo ya Aramagedo isanayambe . Conco , anapewelatu kuchula Mulungu kapena ciliconse cokhudza Mulungu . DZIKO : UNITED STATES Akhiristu onse anali kutsatila zimene Yesu Khiristu , Woyambitsa Cikhiristu , anali kuphunzitsa . Komabe , kukhala aubwenzi pamene mukufotokoza cifukwa cimene mwafikila pa khomo la munthu , nthawi zambili kumathandiza kucepetsa nkhawa kapena ukali umene mwininyumba angakhale nawo . Ndipo kodi si Paulo anauza Timoteyo kuti azimwako “ vinyo pang’ono ” ? ( 1 Tim . Pamene tinali kuyang’ana cigwa , anatiuza kuti tiŵelenge 1 Samueli 17 : 1 - 3 . Masutikesi anga ine ! Mwina Mkristu angakumbukilenso zimene acicepele anali kuona kuti ndi khalidwe loipa m’ma 1950 ndi zimene zikucitika masiku ano . Niyamikila kuti abale analeza mtima poniphunzitsa nchitoyo . Zaka zoposa 2,600 zapitazo , Mfumu Nebukadinezara wa ku Babulo anaimika fano lina lalikulu la golide , ndipo anapeleka lamulo lakuti aliyense ayenela kuwelamila fanolo ndi kulilambila . Kwa zaka pafupi - fupi 100 tsopano , takhala tikuona kukwanilitsidwa kwa ulosi wopezeka pa 2 Timoteyo 3 : 1 - 5 . Mose “ anayang’anitsitsa pamphoto imene adzalandile . ” Anthu ena angavutike kufuna - funa makiyi ao kapena magalasi ao a m’maso pamene mwina ali nao pafupi . Analeka kuyenda motsatila za thupi ndi kubwelela m’njila yolongosoka . — 2 Akor . Panthawi imeneyo io analalikilapo ku dela lina la ku midzi . Mulungu analenga Adamu ndi Hava ndi kuwapatsa mphatso yobeleka ana angwilo . ( 1 Pet . 1 : 13 - 15 ) Tikatelo , tidzakhala na cikhulupililo na nzelu yocokela kwa Mulungu . Koma anafotokoza bwino . A Inoki : Zikomo kwambili cifukwa coŵelenga bwino . Aisiraeli anacita mantha na mtambo wakuda , mphenzi , na zizindikilo zina zocititsa mantha zocokela kwa Mulungu . Pamene maluŵa akula , amawadulila bwino kuti apitilize kukula mmene iye afunila . Labwino Kwambili Kuposa Dayamondi ( kuona mtima ) , June Ganizilani zinthu zokondweletsa zimene tidzamva kwa iye . Iye anagonjetsa Babulo ndi kupeleka cilengezo cakuti : “ Yehova . . . wandituma kuti ndim’mangile nyumba ku Yerusalemu . . . Lemba la Yakobo 4 : 8 limafotokoza mmene mungacitile zimenezo . “ Ngati ndiwe wokhulupilika m’cikwati , umalolela kulakwilidwa . ( Mac . 15 : 37 - 39 ) Patapita zaka , Maliko anali ku Roma kuthandiza Paulo amene anali m’ndende . Polembela Akristu a ku Kolose , Paulo anachula zabwino zimene Maliko anali kucita . Mkazi wake , Annalou , anavomeleza ndipo anati : “ Kuŵelenga zitsanzo za m’Baibo kwatithandiza . 22 : 39 . Kodi timapemphela kwa Atate wathu wacikondi wakumwamba tsiku lililonse , kumuyamikila cifukwa cotikonda na kutipatsa mwayi wokhala m’gulu lake ? Mlongo wina wa ku Britain anati : “ Pambuyo pocita maphunzilo a za cikhalidwe ku yunivesite , n’nayamba kufunitsitsa kuti zinthu zisinthe . Baibo imakambanso zina zokhudza ciukililo copita kumwamba . Imati : “ Sitikufuna kuti mukhale osadziŵa za amene akugona mu imfa , . . . Baibo imakamba kuti kufatsa kuli na mphamvu yaikulu . A Inoki : Zithunzi zimenezi zikuonetsa Mboni za Yehova zimene zikugwila nchito yolalikila padziko lonse . M’mashopu ogulitsa mabuku mumapezeka mabuku ambili - mbili othandiza , ndipo ndalama madola ambili - mbili zimaonongedwa kupanga mabuku amenewa . Cifukwa Cake Timacita Mgonelo wa Ambuye Ena anaphunzila cinenelo catsopano kuti athandize mpingo kapena gulu la cinenelo cimeneco . Comalizila , mudziona nchito iliyonse yocokela kwa Yehova kuti ndi umboni wakuti ali ndi inu . Anafunanso kuti mfundo zake zizititsogolela komanso kuti tizindikile kuti Yesu anatiphunzitsa mfundo zapamwamba kuposa za m’Cilamulo . Kodi kuseka kwa Sara kuonetsa kuti analibe cikhulupililo ? Limbikitsani amene akukumana ndi mavuto Ambili pamsonkhanowo anali na cidwi ngako cofuna kumvetsela . “ Panthawi yovutayi , ndinacondelela Yehova kuti athandize banja langa kukhalabe lokhulupilika . Zimenezi n’zosadabwitsa cifukwa Yesu anati : “ Anthu adzakupelekani ku cisautso ndipo adzakuphani . Mitundu yonse idzadana nanu cifukwa ca dzina langa . ” Ndipo cinenelo cimatithandiza kudziŵa kuŵelenga , kulemba , kukamba , ndiponso kumvetsa zimene zikukambidwa . Koma pokhapo ngati mwakambilana ndi m’bale wanu maulendo angapo ndipo mwalephela kukhazikitsa mtendele ndi pamene ( 3 ) mungauze akulu za vutolo . 9 : 19 , 20 ; 13 : 5 , 14 - 16 ; 14 : 1 ; 17 : 1 , 2 . Iwo anali kufuna kum’cotsela nkhongole yonse ndi kumupempha kuti awakhululukile . Mwacitsanzo , Yehova amafuna kuti tizipewa macimo akuluakulu monga ciwelewele , kulambila mafano , kuba , kulanda , kupha , ndi kukhulupilila mizimu . — 1 Akor . Sayansi ya zamankhwala yathandizako kuti odwala asamamwalile msanga . Kodi pali m’bale wacikulile amene ni bwenzi lanu limene mumafuna kutengela citsanzo cake ? Iye ananituntha kuti niyambe maseŵela a nkhonya . Pali mavuto amene lomba sitingawapewe kapena kuwathetsa . ( Afilipi 4 : 13 ) Tsiku lililonse , Yehova amanipatsa mphamvu zofunikila kuti nicite zinthu “ zofunika . ” Mwina Inoki adzatiuza ngati zimene tiganiza zokhudza imfa yake n’zoona . Pamene anali mtsikana , iye anali kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . Koma ataloŵa m’banja , anasamuka kupita pacilumba cina . Nditakhalako kwa miyezi yocepa , ndinaloledwa kucoka . Sindikukaikila kuti zocepa zimene takambilanazi , zakuthandizani kuona kuti zimene Mboni za Yehova zimakhulupilila ponena za Ufumu zimacokela m’Baibulo . Ndinali kulakalaka kupezako munthu wa conco , koma zimenezo sizinacitike . ” Kodi mungadziŵe bwanji zimene Yehova afuna ? Popeza kuti Mboni za Yehova ndi alaliki ndi aphunzitsi odzipeleka , io amakhulupilila kuti anapeza coonadi . Ndipo zimenezi zimawalimbikitsa kudzipeleka kuti azilalikila kwa anthu amitundu yonse ndi a zikhalidwe zosiyanasiyana . Cipinda cimene tinalimo cinali ndi mabedi ambili m’mbali mwa zipupa . ( Eks . 7 : 6 ) Koma n’kutheka kuti pambuyo potsogolela Aisiraeli opanduka kwa zaka zambili , iye analema komanso anakhumudwa na zocita zawo . Anacita kuvomeleza kuti : “ Ndikulila mofuula cifukwa ca kuvutika kwa mtima wanga . ” ( Sal . Cifukwa cakuti ciyembekezo cawo cinali cotsimikizika , amuna ndi akazi amenewa anali ofunitsitsa kukhalabe okhulupilika kwa Mulungu olo akumane ndi mavuto abwanji . Fotokozani madalitso amene wacicepele amapeza akadziikila zolinga zauzimu akali wamng’ono . kanjele ka mpilu ? Iwo atumikila ku United States . Mu 2005 , m’dzikolo mutawomba cimphepo camphamvu cochedwa Hurricane Katrina , iwo anagwilako nchito m’gulu lothandiza pakagwa masoka . NYIMBO : 51 , 135 Bwanji ngati ayamba kufika pa misonkhano , kodi ndi nyimbo ziti zimene adzizaimba ? Ndi mabuku otani amene angagwilitsile nchito ? 28 : 19 , 20 ) Kuwonjezela apo , timapeleka ulemelelo kwa Yehova mwa khalidwe lathu labwino . Masiku ano , anthu amagwilitsila nchito cinenelo ca Cikatalani , ndi zinenelo zina zofanana naco m’zigawo za ku Andorra , Alicante , zilumba za Balearic , ndi ku Valencia . ( Yelekezelani ndi Luka 14 : 16 - 20 . ) Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikila mphatso imeneyi yocokela kwa Yehova ? Nanga aliyense wa ife angacite ciani kuti athandize kukongoletsa paladaiso ameneyu ? Koma patapita nthawi ing’ono , tinazoloŵela umoyo watsopano umenewo cakuti zinthu zimenezo sizinaonekenso monga n’zovuta . ” Tisaiwale kuti Yehova Mulungu amaona zonse . Davide anali kulakalaka kumanga nyumba ya Yehova . M’nkhani ino , tidzakambilana mmene tingavulile umunthu wakale ndi cifukwa cake tifunika kucita zimenezi mwamsanga . Mulungu anaonetsa cikondi cacikulu potumiza mwana wake padziko lapansi kuti adzatifele . Mau a Mulungu ndiye gwelo la coonadi . 9 : 6 . “ Umutulile Yehova nkhawa zako , Ndipo iye adzakucilikiza . ” — Salimo 55 : 22 Nanga tingalemekeze bwanji cikumbumtima ca ena ? Koma , kodi Yesu anacoka bwanji ku cipululu kupita ku kacisi ku Yerusalemu ? M’fanizo lokhudza kapolo wokhulupilika , Yesu anatsindika mfundo yakuti odzozedwa ocepa amene apatsidwa nchito yodyetsa anchito apakhomo m’masiku otsiliza ayenela kukhala okhulupilika ndiponso anzelu . 4 Zimene Baibo Imakamba pa Nkhani ya Moyo na Imfa Mwacitsanzo , tinafunika kuphunzila moseŵenzetsela ziwiya zimene poyamba sitinali kuzidziŵa . 4 : 14 ) Ndipo anthu ena anadziŵika ndi maudindo awo akuuzimu . Kodi mwakonzekela kucita zimenezo ? Ŵelengani Salimo 45 : 10 , 11 . Kodi mau a pa Aroma 14 : 21 angatilimbikitse bwanji kulemekeza cikumbumtima ca ena ? Ndipo amene anali kutsutsa zimene atsogoleli anali kuphunzitsa , anali kulangidwa mwankhanza . ( Miyambo 23 : 20 ) Kumwa moŵa mopitilila malile kumawononga thanzi la munthu , vikwati vimagwedezeka na kutha , ndipo anthu mamiliyoni amafa mwamsanga caka ciliconse cifukwa ca moŵa . Pambuyo pokamba za Inoki , Paulo anati : “ Popanda cikhulupililo n’zosatheka kukondweletsa Mulungu . ” Akristu amene anali ku ndende ku Nicaragua , anali kupatsilana pepala ndi pensulo iyi kuti alembe ciŵelengelo ca anthu omwe afika pa cikumbutso mu selo lililonse Koma Yehova anatambasula dzanja lake ndi kuthandiza banja lokhulupilika limeneli . Kodi zimenezi zinali kudzacitika liti ? Conco , mkulu wa atumiki a Farao ophika mikate anali ndi udindo wapamwamba . kunyada ? Kodi Yehova amatiphunzitsa bwanji moleza mtima kuti tizitha kudzilanga tekha ? 22 “ Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi ? ” Pasondo ndinali kukhala pa gulu la oimba kwaya ku chalichi . Kunena zoona , ngati tonse ticitila anzathu zabwino , kaya akhale a mumpingo kapena a m’gawo lathu , timathandiza kuti mumpingo mukhale mgwilizano . ( Afil . 121 : 1 , 2 . Mosiyana ndi Blessing , poyamba Yosefe sanacitilidwe nkhanza . Mofananamo , Yesu , Mutu wa mpingo , ndiye mtsogoleli wa anthu amene ali m’pangano latsopano . — Aef . Ganizilani citsanzo ca Jaime amene anali wankhonya . Atatsala pang’ono kufa , iye anafuula mwamphamvu kuti : “ Ndakwanilitsa cifunilo canu ! ” — Yoh . Ngakhale n’conco , thandizo lilipo . Ambili a ife takhala maso mwakuuzimu kwa zaka zambili . Dikishonale ina inanena kuti kusankhana mitundu kumatanthauza “ kusankha anthu kapena kudana nao cifukwa cakuti si a mtundu wathu . ” Kodi mungakonze zopita nao muulaliki kuti aone cimwemwe cimene muli naco cifukwa cotumikila Yehova ? Yakobo 4 : 17 Nthawi zina , zingakhale zovuta kulalikila anzanu kusukulu . Sanali kuganizila za iye yekha basi , koma anali kuganizila kwambili za Atate wake wakumwamba . M’nkhani yotsatila tidzakambilana njila zina zimene zingathandize makolo okalamba ndi ana ao . [ Cithunzi papeji 20 ] Iye analonjeza Mfumu Davide kuti nthawi zonse adzam’tsogolela ndi ‘ kumuyang’anila . ’ Ngakhale kuti Solomo anakamba kuti ukalamba ndi nthawi yovuta , Yehova amayamikila zonse zimene Akristu acikulile amacita pom’tumikila . Zimenezo zinawathandiza kupita patsogolo , ndipo tsopano ndi apainiya aluso . 83 : 18 . Mkazi wanga , Mairambubu anamva mau amenewa pamene anali m’basi pa ulendo . Iye anali ndi cikhulupililo mwa Yehova ngakhale kuti anadziŵa kuti kucita zimenezo kunali kuika moyo wake pangozi . — Yoswa 2 : 9 - 13 ; 4 : 23 , 24 . Takuya anapita patsogolo cakuti anakhala mpainiya wa nthawi zonse , ndipo tsopano akutumikila pa ofesi ya nthambi . Conco , onse aŵili amafunika kucitapo kanthu kuti ubwenzi ukhalepo . Nitakwanitsa zaka 16 , mnzanga wina wa paubwana , dzina lake Jorge , anabwela kunyumba kwathu . N’ciani cimene atumiki okhulupilika a Yehova anaphunzila panthawi ya mavuto ? N’cifukwa ciani mau akuti “ paladaiso wauzimu ” ndi akuti “ kacisi wauzimu ” ndi osiyana ? Koma mipukutuyo inali yovuta kunyamula . Banja lina limene linali kutumikila panthambi yaing’ono ku Central America , linapemphedwa kukakatumikila ku nthambi yaikulu kwambili ku Mexico . Mosakayikila inamulimbikitsa . Umboni wa zimenezi ni wakuti kalata yacitatu ya Yohane inalembedwa m’Baibo n’colinga cakuti izilimbikitsa ena ‘ kutsanzila zabwino . ’ Paja Yesu anati : “ Kumene kuli cuma canu , mitima yanunso idzakhala komweko . ” — Luka 12 : 34 . Patapita nthawi , anabatizidwa ndi kukhala mtumiki wa nthawi zonse . 9 : 36 , 39 ) Mariya , mlongo wa mumpingo wa ku Roma , anacitila Akhiristu anzake nchito zambili . Tingapindule bwanji ndi mphamvu yokwanitsa kuganizila zinthu zimene sitinazionepo ? A Doris anabatizika mu 2010 , ndipo tsopano amatsogoza maphunzilo a Baibulo angapo . ( Agalatiya 6 : 10 ) Ngati tithandiza ena , tidzakhala osangalala ndipo ‘ tidzapitiliza kubala zipatso m’nchito iliyonse yabwino . ’ — Akolose 1 : 10 ; Machitidwe 20 : 35 . 19 : 7 - 11 ) Tiyenela kutsatila zimene timaphunzila . Zimenezo zinandithandiza kukhalanso ndi cidalilo , ndipo tsopano nditumikilanso monga mkulu . ” 14 : 1 ) Ndipo mzimu wa Mulungu umawacititsa kufuula kuti , “ Abba , Atate ! ” 1 : 19 . Sin’nafune kuti nioneke ngati munthu wosayamikila pa kukoma mtima kumene Mulungu wanionetsa . MUKAMVA liu lakuti “ cilango , ” mumaganizila za ciani ? ALENDO ocezela malo anamva njala . Kupyolela m’Mau ake , Yehova amatilimbikitsa ‘ kumuyandikila , ’ ndipo amatilonjeza kuti tikatelo , ‘ iyenso adzatiyandikila . ’ ( Yak . Kodi Moto Unali “ Kunyamuliwa ” Bwanji M’nthawi Zakale ? Atatsiliza kulalikila m’ziguduli , odzozedwa amenewa mophiphilitsila anaphedwa mwa kuikidwa m’ndende kwa kanthawi . Kanthawi kameneka kanaimila masiku atatu ndi hafu . Motelo , Komiti Yomasulila Baibulo la Dziko Latsopano inakhazikitsidwa , ndipo abale a m’komiti imeneyi anali kutulutsa zigawozigawo za Baibuloli kuyambila mu 1950 mpaka mu 1960 . Zimenezi zathandiza kuti Mboni za Yehova padziko lonse lapansi zizimvetsetsa “ cilankhulo coyela ” ca m’Baibulo ndi kukhala ogwilizana . — Ŵelengani Zefaniya 3 : 9 . Yehova anathandiza Yesu ndi kum’tsogolela m’njila zodabwitsa . Pali malangizo pamawebusaiti ambili - mbili , alangizi ochuka pamapulogilamu apa TV , makambilano a akatswili odziŵa za maganizo a anthu , aphungu a zacikhalidwe , ndi akatswili olemba mabuku . Uwasunge bwino cifukwa iwo ndiwo moyo wako . ” Baibo imaonetsa kuti anafunika kuyembekezela . Iye anandifunsa kuti : “ Kodi Yesu ndi atumwi ake anafunikila galimoto kuti acite utumiki wa nthawi zonse ? ” 8 : 28 ) Ngati timvela malamulo a Yehova na Yesu , iwo adzapitiliza kutikonda . Muzikoka mpweya wokwanila M’malo mwake , Adamu anauzidwa kuti adzabwelela ku nthaka . Adamu anakondwela kwambili na mkazi wake wokongola , ndipo anamucha dzina lakuti Hava . Kodi pali zinthu zina zimene mungacite kuti kulambila kwanu kwa pabanja kukhala kosangalatsa ? ( a ) Ni madalitso anji amene timapeza ngati ticita zopeleka zocilikiza Ufumu wa Mulungu ? Kodi mlongo wina wacitsikana anatsatila bwanji zimene cikumbumtima cake cophunzitsidwa bwino cinamuuza ? M’bale wina amakumbukila zimene zinacitika pamene anali mnyamata . 18 : 1 - 6 ) Kuti awateteze kwa “ woonongayo , ” mwamsanga Mose “ anaitana akulu onse a Isiraeli ndi kuwauza kuti : . . . Komanso ganizilani za anthu acidwi mamiliyoni ambili amene anapezeka pa Cikumbutso . Yesu anapeleka citsanzo ca mmene tingayendele ulendo umenewu . Iye anagwilitsila nchito citsanzo ca Yesu , amene anafa monga munthu , koma anaukitsidwa monga munthu wamzimu ndi kupita kumwamba . Malinga ndi Chivumbulutso 14 : 6 , 7 , kodi angelo amawathandiza bwanji anthu a Mulungu masiku ano ? NYIMBO : 45 , 70 Ngati mwamuna ndi mkazi amakondanadi , cikwati cao cidzakhalabe colimba ngakhale atakumana ndi mavuto aakulu . ( Salimo 51 : 15 ) Tikamagwilitsila nchito mphatso yathu ya kulankhula mwanjila imeneyi , ndiye kuti tikuyamikila Yehova cifukwa cotipatsa mphatsoyi . Woyang’anila ndendeyo ayenela kuti anali msilikali wopuma pa nchito . Ponena za kuphedwa kwa Yesu ndi zigaŵenga ziŵili , Uthenga wabwino umati : “ Ayudawo . . . anapempha Pilato kuti opacikidwawo awathyole miyendo ndi kutsitsa mitemboyo . ” — Yohane 19 : 31 . ‘ Mofanana ndi munthu amene mayi ake amamutonthoza , inenso ndidzakutonthozani anthu inu . ’ ” — Yesaya 66 : 12 , 13 . 13 , 14 . ( a ) N’ciani cimacititsa kuti anthu a Mulungu afooke ? 62 : 8 . 4 : 23 , 24 ) Kudzilanga wekha ni mbali yofunika kwambili ya umunthu watsopano . 1 : 9,10 . Kwa ena , cimakhala covuta kupeleka moni kwa anthu cifukwa cosiyana mtundu , cikhalidwe , udindo , msinkhu , kumene anakulila , kapena cifukwa cakuti si mwamuna kapena mkazi mnzawo . 136 : 1 , 5 - 9 . Kodi ningaciteko bizinesi iyi ? Anthu a mtima wapacala , amakonda kukamba mau acipongwe akapsa mtima . Fotokozani zitsanzo zoonetsa madalitso amene timapeza ngati ticitila cifundo anthu amene timapeza mu ulaliki . 12 : 14 . Zaka 100 za Ulamulilo wa Ufumu wa Mulungu Onani Buku la pacaka la Mboni za Yehova 2014 , masamba 12 - 13 . Mau oyamba m’Baibo ya uthenga wabwino anaonetsa kuti Lefèvre anali wofunitsitsa kuti anthu onse akhale na Baibo m’cinenelo cawo Kusinkha - sinkha zimenezi kumatipangitsa kuyamikila kwambili mlengi wathu ndi kum’tumikila mmene tingathele tikali moyo . — Mlal . Cifukwa ca cifundo , Yesu anayamba kulankhula ndi munthu amene anayamba kudwala Yesuyo asanabadwe padziko . — Ŵelengani Yohane 5 : 5 - 9 . Lemba la Afilipi 2 : 4 linandithandiza kuti sindiyenela kuganizila kwambili za ine ndekha kapena zokhala ndi famu yaikulu . Pofuna kuthandiza ofalitsa atsopanowa nthambi ya ku France inasankha oyang’anila oyendela oyamba mu 1948 . N’nadzifunsa kuti , ‘ Kodi malamulo amenewa anakhalako bwanji ? Woyambitsa nyuzipepala imeneyi , analonjeza kuti zolembedwa zake zizikhala “ zoona zokhazokha basi . ” Kuti mudziŵe zambili , onani buku yakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse yofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . Mwacitsanzo , abale okalamba amene atumikila kwa nthawi yaitali angapemphedwe kutula pansi udindo wao kuti acilikize abale acinyamata amene apatsidwa udindowo . Kugwilitsila nchito dzina la Mulungu kokha sikungatiyanjanitse ndi Yehova . Cifukwa cakuti Davide nayenso anakumanapo ndi mavuto ocokela kwa atumiki ena a Mulungu . Mwacitsanzo , mvelani zimene munthu wina dzina lake Michael anali kucita akaona Mboni za Yehova . Iye anasintha kwambili . Zimenezi zimatikumbutsa mau apa lemba la Numeri 16 : 5 . ( Kodi mzimu woyela ungatithandize bwanji ? Timaphunzilanso buku lakuti “ Khalanibe M’cikondi ca Mulungu ” n’colinga cakuti tiwathandize kukonda kwambili Yehova ndi miyezo yake . Anthu ena amakhala m’cikwati cabe cifukwa cokakamizidwa na acibululu awo kapena anzawo . Tikamaona Yehova monga Wotiumba wathu , timayamba kuona abale ndi alongo athu moyenela . 45 : 3 , 4 . 3 : 5 , 6 ) Musaiŵale kuti cilango ca Yehova cimaonetsa cikondi cake na nzelu zake zopanda malile . Julie anati : “ Msonkhano utatha , tinapemphela kwa Yehova kuti tikhale olimba mtima kuti tikapite ku Taiwan . ” ( Luka 8 : 45 - 47 ) Pakumva izi , mzimayi uja ali nje nje nje ndi mantha , anagwada kwa Yesu “ ndi kumuuza zoona zonse . ” — Maliko 5 : 33 . Kodi ndimayesetsa kuuzako ena za Mulungu ? 6 Kodi Inatha Nchito Kapena Imakambilatu Zinthu Zimene Anthu Akalibe Kuzitulukila ? Mwakucita zimenezo , Yesu anaonetsa kuti Mulungu ndi woyenela kulamulila . Jairo atamucita opaleshoni , ndimakumbukilabe mmene anali kulilila usiku uliwonse cifukwa ca ululu . Conco , ngakhale tikumane ndi mavuto kapena mayeselo , tifunika kuyesetsa kukhala “ ndi mtima wodikila . ” Ndiyeno , Davide akuuza anthuwo kuti : “ Nchitoyi ndi yaikulu cifukwa cinyumba cacikuluci , si ca munthu ayi , koma ndi ca Yehova Mulungu . ” — 1 Mbiri 28 : 1 , 2 , 6 , 11 , 12 ; 29 : 1 . 3 : 13 ) Lemba la Salimo 37 : 11 limati : “ Anthu ofatsa adzalandila dziko lapansi ndipo adzasangalala ndi mtendele woculuka . ” Sukulu imeneyi inali kucitila zinthu zina pamodzi ndi Grand Hotel . ( Gen . 6 : 9 ) Iye anauza Nowa kuti adzawononga dziko loipa la pa nthawiyo , ndipo anamuuza zimene anayenela kucita kuti apulumutse banja lake . ( Gen . Koma poyembekezela kuti mpata ukapezeke , muzim’pemphelela m’bale wanuyo . ‘ Inu anyamata ndi inunso anamwali . . . . tamandani dzina la Yehova . ’ — SAL . Iye analemba kuti : “ Pitilizani kuphunzitsana ndi kulangizana mwa masalimo , nyimbo zotamanda Mulungu , ndi nyimbo zauzimu zogwila mtima . Pitilizani kuimbila Yehova m’mitima yanu . ” — Akol . Ngati mlandu wathu sunayende bwino ku makhoti aang’ono , timapita ku makhoti aakulu padziko lonse . N’cifukwa ciani nili na moyo ? ’ Tingacite ciani kuti tizikhulupilila kwambili Yehova ndi kulimbitsa ubwenzi wathu ndi iye ? Apa m’pamene atate anayamba kuphunzila Baibo . Pamene munayamba kuphunzila Baibulo na wa Mboni za Yehova , muyenela kuti munamvela monga mmene munthu amene wapeza golide wambili amamvelela . Ngati ena akukhumudwitsani , kodi n’ciani cingakuthandizeni kukhalabe wacimwemwe potumikila Yehova ? Tsopano tiyeni tibwelele m’mbuyo miyezi yambili zimenezi zikalibe kucitika . ( Miyambo 24 : 14 ) Kuonjezela apo , phunzitsani ana anu kuti azipita mu utumiki kaŵilikaŵili . Ife titayankha kuti inde , anapitiliza kuti : ‘ Ndinali kudziŵa kuti tsiku lina mudzafika pa nyumba panga . Ndipo atumiki a Mulungu onse angapidule ndi citsanzo ca alongo amenewa . ( 1 Mafumu 17 : 1 ) ( 2 ) Eliya anali ndi cikhulupililo cakuti Yehova adzamusamalila pamodzi ndi atumiki ena panthawi ya cilalaco . Si canzelu kutumila ena zimene mwaŵelenga , ndi kupempha kuti mumve maganizo ao . Kucita zimenezo kungapangitse kuti nkhani yoipa imeneyo ifalikile kwambili . Kuphunzila Baibulo kwandithandiza kukhala ndi umoyo wabwino ndi kukhala mwamtendele ndi anthu onse . ( 1 Pet . 4 : 3 , 4 ) N’zoona kuti timayesetsa kuti tisawakhumudwitse . Poyamba , kupeza nchito kunali kovuta . Vuto lina linali lakuti banjali linali kungokhalila kusamukasamuka . Mwina pafunikanso abale odzipeleka kuti athandize kugwila nchito yomanga imene ikucitika kudela lanu . Motelo , Yehova adzakweza ulamulilo wake ndi kuyeletsa dzina lake , popeza iye anati : ‘ Ndidzacititsa kuti mitundu yambili ya anthu indidziŵe , ndipo io adzadziŵa kuti ine ndine Yehova . ’ — Ezek . Ndipo kugwila nchito imeneyo kunali ngati cakudya cake . — Yoh . 4 : 31 - 34 . Cofalitsa cimeneci cingakuthandizeni kuti mupindule kwambili mukamaŵelenga mabuku a Uthenga Wabwino . — Yohane 14 : 6 . Mwanjila imeneyi , omasulila Baibo ya King James Version anaonetsa kuti anali kudziŵa kuti dzina la Mulungu lifunika kupezekanso m’malemba ochedwa Cipangano Catsopano . Mtumwi Paulo anali kudziŵa Akhristu ambili a m’mipingo ya ku Asia Minor na ku Europe . 65 : 13 ) Mwacitsanzo , Nsanja ya Mlonda yofalitsidwa m’zinenelo zoposa 210 , imafotokoza maulosi a m’Baibulo . Imatithandiza kumvetsetsa zinthu zozama za kuuzimu ndi kutithandiza kutsatila mfundo za m’Baibulo paumoyo wathu . 97 : 10 ; Miy . Dziko lapansi linapangidwa moyenelela kuti pakhale zamoyo . Muzitumilako foni mnzanu wa m’cikwati nthawi zonse mukakhala kunchito kapena pamene muli kwina 18 , 19 . ( a ) Kodi zocitika za m’nthawi ya atumwi zinatheketsa ciani ? ( b ) Ndi mapindu otani amene inuyo mudzapeza cifukwa copeleka mapemphelo aciyamiko ? Cikwati cimalimba ngati okwatilana amakonda kulankhula za kukhosi momasuka . Pamene muyesetsa kuti mukwanilitse zolinga zanu , ‘ muziyembekezela moleza mtima . ’ Tingaphunzilekonso citundu cina , ndi kupita kumene kuli alengezi a Ufumu ocepa m’dziko lathu kapena m’dziko lina . — Mac . Atate wathu Wakumwamba ndi wotsimikiza kuti adzakwanilitsadi malonjezo ake , ndipo kwa iye zili ngati kuti akwanilitsidwa kale . Kodi Zekariya anaona ciani m’masomphenya ake a namba 6 ? Kodi Yesu anathandiza bwanji kuti dzina la Mulungu liyeletsedwe ? PAMENE Antoine Skalecki anali wacinyamata , nthawi zambili anali kukonda kukhala ndi hachi . ( 1 Yohane 4 : 8 ) Yesu analamula otsatila ake kuti ‘ azikondana . ’ ( b ) Tikambilane mfundo zinayi ziti ? Ndipo Mulungu ananenelatu kuti mzindawu udzakhala ‘ bwinja , ndi wopanda madzi ngati cipululu . ’ Mwacitsanzo , mlongo wina dzina lake Renee , anadwala matenda a sitroko komanso anali na khansa , ndipo anali kuvutika na ululu nthawi zonse . Polembela Akhristu anzake , iye anafotokoza cifukwa cake . Iye anati : “ Pakuti cilamulo ca mzimu umene umapatsa moyo mwa Khristu Yesu cakumasulani ku cilamulo ca ucimo ndi ca imfa . ” Cinenelo cacikulu ku Honduras ndi Cisipanishi . Cotelo , Yesu anaphunzitsa anthu zimene Mulungu amafuna , ndipo analamula ophunzila ake kuti agwile nchito imeneyi . Mcitidwe umenewo unabweletsa imfa zambili . Baibulo limati : “ Tsutsani Mdyelekezi ndipo adzakuthawani . ” — Yak . Conco , n’kutheka kuti pano pamene taimilila ndiye pamene Aisraeli anamanga msasa . ’ Posapita nthawi , M’bale Hardaker ananipempha kuti niyambe kuyenda naye mu ulaliki . Amayi anauza a Willie kuti Nkhondo Yaikulu itangotsala pang’ono kuyamba , atate awo ndi alongo awo anamila pamadzi boti yawo itagunda bomba yocheledwa pamadzi ku North Sea . 72 : 12 , 13 . Nthawi zonse pamene muuzako anthu amene amakusamalilani ndi ena uthenga wabwino , mumalemekeza Mulungu . Kristu Ndiye Mphamvu ya Mulungu 4 : 8 , 9 ; Chiv . 12 : 12 ) Cimwemwe cimene munthu angapeze cifukwa cogwila nchito yakuthupi n’cosakhalitsa tikaciyelekezela na cimene munthu amapeza ngati aphunzitsa anthu za Mulungu kuti akapeze moyo wosatha . Ngati timakonda anthu ndi kuwaganizila , timasankha bwino mau pokambilana nao . Iye panthawi ina anaona kuti sangakwanitse kugwila nchito imene anapatsidwa . Kugwilizana kumatanthauza kucita zinthu monga woyendetsa ndeke na wom’thandiza wake amene onse ali na colinga copita ku malo amodzi Paulendo wotsatila mungakambilane zoonjezeleka . Ndi mfundo ziti zimene zimatithandiza kudziŵa cifukwa cake Yehova anakantha Azariya ndi khate ? Ndiyeno anapempha mwamuna wake kuti abeleke ana kupitila mwa wanchito wake wamkazi , Hagara . Cilamulo cimeneco cinaonetsa mmene Yehova amaonela mavalidwe amene sasiyanitsa amuna ndi akazi . Mavalidwe amenewo afala kwambili masiku ano . Izi zinamveka ngati kuti pamene Yakobo anatenga udindo wokhala woyamba kubadwa , analoŵa pa mzela wa makolo a Mesiya . — Mat . Tiyenela kufufuza , kufunsilako kwa ena , ndi kupemphela . Kenako , ticite zimene mzimu wa Mulungu ukutitsogolela . N’ciani cimakucititsani cidwi na kulimba mtima kwa Yosefe ? N’cifukwa ciani tingakhale na cikhulupililo cakuti Yesu amatimvela cifundo masiku ano ? M’nkhani ino , tikambilana zitsanzo zocepa zoonetsa mmene Mulungu wakhala akutsogolela anthu ake . Ngati tadwala pamakhala zithandizo za mankhwala zosiyanasiyana , ndipo tili ndi ufulu wosankha cithandizo cimene tifuna . Baibulo limati : “ Ona munthu wosalakwa ndipo yang’anitsitsa munthu wolungama , Pakuti tsogolo la munthu ameneyu ndi lamtendele . ” — Salimo 37 : 11 , 37 ; Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . Mtumwi Paulo anamveketsa bwino mfundoyi pamene analalikila gulu la anthu amene anasonkhana ku Areopagi . 16 : 18 . M’bale Lett , anafotokoza kuti cimodzi mwa zifukwa zimene anakonzelanso bukuli n’cakuti mau ake agwilizane ndi a mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lokonzedwanso . Shannon akali kukumbukila mmene anamvela atapezeka pa msonkhano wa cigawo ali ndi zaka 11 , limodzi ndi mng’ono wake amene anali ndi zaka 10 . Pakakhala kusintha kwa conco , tifunika kupatula nthawi yophunzila nkhaniyo mosamala na kuisinkhasinkha . ( Mac . Tangoganizilani cabe za mabuku masauzande - masauzande a zamalamulo amene anthu alemba , komanso maloya na oweluza ambili - mbili amene nchito yawo ni kufotokoza tanthauzo la malamulowo na kuonetsetsa kuti akutsatilidwa . Ndipo imatipatsa ciyembekezo ca zinthu zina zam’tsogolo , ngakhale kuti tifunika kupilila zotulukapo za ucimo . Ngati mufuna , mungapindule ndi pulogalamu yophunzila Baibulo kwaulele ndi Mboni za Yehova . Iye anati : “ Ine na mwamuna wanga tikayamba kuona ngati kuti ena satiŵelengela mu mpingo , timamuuza Yehova mwacindunji m’pemphelo kuti , ‘ Tithandizeni kudziŵa ngati ticita zinthu zimene zikulepheletsa ena kumasuka nase . ’ Koma coumba cimodzi cili bwino - bwino mmene anacipangila . Tsiku lina madzulo , ndinangomva kugogoda pacitseko apo ndili mkati kuyeselela kuponya zibakela pokonzekela ulendo wopita ku China . Tikaphunzitsa acatsopano kukambilana ndi anthu mwa njila imeneyi , iwo adzakonda kwambili ulaliki . ( b ) Mmene Yehova anacitila zinthu ndi Aroni zimatiphunzitsanji ? Tikadzapulumutsidwa , dziko la Satana lidzaonongedwa pa Aramagedo , imene ndi nkhondo “ ya tsiku lalikulu la Mulungu Wamphamvuyonse . ” — Chiv . Tikaona kuti kukonda zinthu zakuthupi kukucititsa cikondi cathu pa Khristu kuzilala , tifunika kukumbukila mau a Yesu akuti : “ Cenjelani ndi kusilila kwa nsanje kwamtundu uliwonse . ” Conco , ophunzila ake sanakaikile kuti iye anali kuwakonda . Ena mwa anthu amenewa kale anali mbala , zidakwa , zigaŵenga , ndipo ena anali kugwilitsila nchito mankhwala osokoneza bongo . N’cifukwa ciani anthu oona mtima anayamba kukana ziphunzitso za cipembedzo m’zaka ma 100 angapo oyambilila ? Ofalitsa 550 anagaŵila zofalitsa 60,000 m’mawiki aŵili cabe . Mosiyana ndi anthu , Mulungu amadziŵa zonse . “ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ” — MATEYU 22 : 39 . Ndife otsimikiza kuti “ nthawi ya ciweluzo ” yafika . Mwacidule , kodi mungakonde ana anu kutengela citsanzo canu ? ( Miy . 2 : 4 , 5 ) Caciŵili , tiyenela kugwilizanitsa zimene taphunzila ndi zimene tikudziŵa kale ndi kuona mmene zingatipindulitsile . Ciphonaco cinagwa pansi cafufumimba . Mwacitsanzo , Abulahamu ndi Loti , onse anali ndi ziŵeto zambili , ndipo abusa ao anayamba kukangana cifukwa ca kucepa kwa malo odyetselako ziŵeto . Tiyeni tione njila zitatu . Olamulila m’dzikoli amacita zinthu mwadyela ndipo amaumilila maganizo ao , io akana kutsogoleledwa ndi Mulungu . Nthawi zambili mkazi wanga anali kulila , ndipo ndinali kulephela kumutonthoza . ( Yes . 46 : 5 - 7 ) Mosiyana ndi milungu imeneyo , Yehova anauza anthu ake Aisiraeli kuti : “ Inu ndinu mboni zanga , . . . Ndinu mtumiki wanga amene ndakusankhani kuti mundidziŵe ndi kundikhulupilila , komanso kuti mumvetse kuti ine sindinasinthe . Kodi Paulo anali wotsimikiza mtima za ciani ? Nanga mau ake kwa Timoteyo anaonetsa bwanji zimenezi ? ( Mat . 24 : 45 - 47 ) Nkhaniyo inafotokoza kuti kapolo wokhulupilika ndi Bungwe Lolamulila , ndipo “ anchito ake apakhomo ” ndi anthu onse amene amadyetsedwa mwakuuzimu , kaya ndi odzozedwa kapena a “ nkhosa zina . ” ( Yoh . Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Ngati inu mudzapilile , mudzapeza moyo . ” Mwacitsanzo , kuyambila kalekale anthufe timafunikila cakudya , zovala , ndi pogona . Mlongo wina dzina lake Linda , * atasamalila makolo ake amene anali kudwala mpaka pamene anamwalila , anaona kuti n’zoona Yehova amalimbitsa . Kapena kodi n’cifukwa cakuti analibe cithunzi bwino - bwino , mwina anangolephela kuzindikila bwino ? Adzabzala minda ya mpesa n’kudya zipatso zake . ” Koma cifukwa ca kudzicepetsa , anali kuwafotokozela cifukwa cake afunika kucita zimene awauza . Tiyenela kudziŵa nthawi yabwino imene tiyenela kukamba , zimene tiyenela kukamba , ndi mmene tiyenela kukambila . Munthuyo akayankha mungakambe kuti : “ Amuna ambili amapeza ndalama zoposa zimenezo , koma mabanja ao sakhutila nazo . Mukamayangana kuthambo usiku , dzifunseni funso ili : Kodi mphamvu imene imacititsa cilengedwe kupitilizabe kukula imacokela kuti makamaka ? N’tangotsiliza kuŵelenga , n’nakomoka . N’nali n’sanajaile nyengo yotentha , ndipo n’nalimbana ndi vutoli kwa nthawi yaitali . Ndidzakwanilitsa malonjezo anga kwa Yehova , pamaso pa anthu ake onse . ” — Sal . Ngati n’conco , mwamsanga funsani Mboni za Yehova . ( Yesaya 46 : 10 ) Tikamatsatila malangizo a Yehova , timapindula na nzelu zake zosayelekezeka ndi luso lake lodziŵa za mtsogolo . — Yesaya 48 : 17 , 18 . Poona zimenezi , mngeloyo anati : “ Usaope Mariya , pakuti Mulungu wakukomela mtima . ” Nkhondo yoopsayi inali ciyambi ca nyengo imene anthu ambili anaphedwa pa nkhondo zosiyana - siyana kuposa nthawi ina iliyonse m’mbuyomu . Cokondweletsa n’cakuti , usikuwo sindinali nao . Makolo , tikuyamikilani kuti mumacita khama kuphunzitsa ana anu cifukwa cakuti mumawakonda kwambili . 3 : 17 ; 17 : 5 ) Apa Mulungu anayamikila Yesu na kumtsimikizila kuti anali kucita zabwino . Kuciyambi kwa utumiki wake , yekha anakwanitsa ‘ kuthamangitsa onse amene anali na nkhosa na ng’ombe ndipo anawatulutsa m’kacisimo . Woyang’anila dela wina analemba kuti : “ Anzanga amadziŵa pamene ndifunikila thandizo . kuletsedwa kwa nchito yomasulila ? Conco , zimene mumakhulupilila zingakhale zosiyana kwambili ndi za anthu ena amene amati ni Akhiristu . Tiyenela kudziŵa kuti zosangalatsa zaucimo n’zosakhalitsa . Atate awo anali Tera , koma amayi awo anali osiyana . Olemba Baibulo Mateyu ndi Luka analemba zimene zinacitika . Nthawi zina , mungaone kuti mavuto amene mwakumana nawo ni aakulu kwambili cakuti simungakwanitse kuwapilila . 1 : 26 , 28 ; 2 : 16 , 17 ) Zinthu zitatu zimenezi n’zimene zinali zofunika kuti cifunilo ca Mulungu kwa anthu ndi dziko lapansi cikwanilitsike . “ Woweluza wa Dziko Lonse ” Amacita Cilungamo Nthawi Zonse , Apr . Cikwati cacikhiristu ciyenela kuyamba ndi mwamuna ndi mkazi , onse aŵili odzipeleka kwa Yehova , ndiponso omukonda ndi mtima wonse . Mumafuna kutsogolela ana anu kuti atumikile Yehova . 22 : 8 ; Sal . Koma ngati pamalilo anga mudzaona munthu wacilendo , mukakambe naye , ndipo conde muŵelenge kabuku aka kabuluu , [ kutanthauza buku lakuti “ Coonadi Cimene Cimatsogolela ku Moyo Wamuyaya , ” lothandiza pophunzila Baibo limene iye analandila zaka zambili m’mbuyomo ] . Mwacitsanzo , dzifunseni kuti , ‘ Kodi ndimakonda kumvetsela nkhani zokambidwa ndi munthu winawake cifukwa cakuti amakamba mfundo zogwilizana ndi maganizo anga pankhani za ndale ? ’ 1 : 14 ) Panthawiyo , anthu a Mulungu adzafunika kukhala ogwilizana kwambili . Kodi mungalipeze kuti ? Ni mapindu ati amene timapeza ngati tionetsa cikondi ? N’zinthu monga ziti zosavuta zimene tingacite polimbikitsa ena ? 5 : 42 ; 17 : 17 ; 20 : 20 ) Buku lake la Mulungu limalangiza akulu mu mpingo kusungitsa ciyelo m’gulu la Mulungu . ( 1 Akor . 5 : 1 - 5 , 13 ; 1 Tim . Iwo angafalitse mabodza amene angacititse asilikaliwo kumenyana okha - okha kapena amene angawacititse kudzipatula kwa asilikali anzawo . PAMENE Adamu ndi Hava analengedwa , io analibe mdani . Kulimbana ndi mavuto a m’banja ATUMIKI a Yehova akhala akuyembekezela kwa nthawi yaitali kukwanilitsidwa kwa maulosi ouzilidwa . Tinayamikila kwambili mzimu wawo wodzipeleka ndiponso thandizo la anzathu a kumalo kumeneko . Zimenezi ziyenela kutilimbikitsa kulemekeza Mwanawankhosa mogwilizana ndi zolengedwa zoculuka zakumwamba zimene zimafuula kuti : “ Mwanawankhosa amene anaphedwa ndiye woyenela kulandila mphamvu , cuma , nzelu , nyonga , ulemu , ulemelelo , ndi madalitso . ” — Chiv . ( b ) Tingawathandize m’njila ziti anthu ocokela ku maiko ena a mumpingo mwathu ? “ Palipano , zacuma zikuyendako bwino . M’bale Rutherford atazindikila kuti M’bale Klein anali kusunga cakukhosi , anamucenjeza kuti asamale cifukwa angagwidwe ndi Mdyelekezi . Kulambila konama kumeneku kunali kofala m’nthawi ya Inoki . ( Yes . 30 : 18 ) Nayenso Mika amene anakamba maulosi okhudza anthu akale a Mulungu anati : “ Ine ndidzadikilila Yehova . ” 3 : 18 ) N’zoona kuti si nthawi zonse pamene mkazi angagwilizane ndi zosankha za mwamuna wake . Paul anazindikila kuti afunika kugwilitsila nchito “ nzelu zopindulitsa ” kuti banja lake lipulumuke . Sikuti zosankha zonse zimene timapanga zimakhala zazikulu . Zimenezo zidzakhaladi zomvetsa cisoni . ​ — Mat . Ndipo walonjeza kuti posacedwapa adzathetsa matenda onse Tingakambe kuti zoipa zina ndi anthu amene amazicititsa . ( Yohane 12 : 31 ) Popanda cisonkhezelo ca Satana dziko latsopano lolungama lidzakhazikitsidwa , ndipo padzikoli padzakhala mtendele wokhawokha . — 2 Petulo 3 : 13 . Tingalimbikitsenso ena mwa kuwayamikila cifukwa ca makhalidwe awo abwino , kapena kukamba mau ‘ olimbikitsa kwa a mtima wacisoni . ’ Tidzaphunzila mmene dipo ndi Mau a Yehova olembedwa , zimaonetsela kuti iye wacitapo kanthu kuti timuyandikile . Kodi timafuna kuti athu aziganiza ciani akaona mavalidwe athu ? Limakambanso zakuti mngelo anamuuza kuti athaŵile ku Iguputo , ndipo patapita nthawi anamuuzanso kuti abwelele kwawo . ( Ŵelengani Zekariya 8 : 23 ; Chivumbulutso 7 : 9 , 10 . ) Kodi ungaleke bwanji kucita miyambo imene yakhalako kwa nthawi yaitali ? Mudzakondwela kudziŵa nkhani zotsatilazi : Masiku ano , atumiki a Yehova amakonda misonkhano ndiponso amaona kuti ndi yofunika kwambili . Yehova anam’tsimikizila kuti lonjezo lake lonena za mwana lidzakwanilitsidwa . Limbikitsani wophunzila kuŵelenga Baibulo lonse m’caka cimodzi n’colinga cakuti alimbitse cikhulupililo cake Muziyenda naye mu ulaliki . Ali pafupi kufika zaka 24 , anasankhidwa kukhala pulofesa wa Ciheberi ku Leipzig . Atagonjetsa Aamaleki , iye anaika zofuna zake patsogolo m’malo momvela Yehova . M’banja , timaonetsa cikondi kwa wina ndi mnzake ndi kucita kulambila kwa pabanja pamodzi mlungu uliwonse Kodi Petulo analandidwa maudindo atacita colakwa cimeneci ? Iye anali kudziŵa bwino kuti anacitilidwa zinthu zambili zopanda cilungamo . 5 : 19 ) Nkhanza zoopsa kwambili zacitilidwa makamaka kwa akazi . Baibulo silikamba ciliconse . Poyelekezela ndi mabiliyoni ambili a anthu amene akhalapo ndi moyo , a 144,000 ndi “ kagulu ka nkhosa ” kocepa . Mapulaneti amayenda mozungulila dzuŵa monga kuti akutsatila bwino - bwino malamulo a pa mseu . Yehova safuna kuti munthu wina aliyense akawonongeke pa ciweluzo cimene cikubwela . Koposa pamenepo , zimene zinacitika mu ulamulilo wa Solomo zimacitila cithunzi mmene zinthu zidzakhalila mu ulamulilo wa Mesiya . — 1 Maf . Ganizilaninso masukulu aumulungu osiyana - siyana . ( Yes . Kumeneko kunali kacisi amene Asamariya anali kucitilako zikondwelelo monga cikondwelelo ca Pasika . Angakambilane zokhudza kugwilana , kupsompsonana , kapena kukhala kwaokha . ( Miy . Tili na cikhulupilillo cakuti , pa nthawi yake yoyenela , iye adzawononga dongosolo loipali . Iye analenga nyenyezi zambilimbili kumwamba ndi zomela zosiyanasiyana zokongola padziko lapansi . — Salimo 65 : 12 , 13 ; 147 : 7 , 8 ; 148 : 3 , 4 . 26 : 69 - 75 . Izi zinam’thandiza kupilila citsutso coopsa . Kupyolela mwa Yeremiya , kodi Yehova anakambilatu ciani ponena za pangano latsopano ? Conco , masiku ano iye akuthandiza kapolo wokhulupilika ndi wanzelu pogwilitsila nchito zinthu zimenezi . N’cifukwa ciani anthu ambili anakhala Akristu ? Ndiponso , ciyembekezo ca Ufumu cimatitonthoza . “ Usayese kucita zimenezo . 29 Kufatsa — Kumaonetsa Nzelu Pali kusiyana kwanji pakati pa ufulu wodzisankhila zocita na udindo wodziŵitsa cabwino ndi coipa ? Mwamuna anali kuloledwa kusudzula mkazi wake cifukwa ca “ vuto linalake . ” ( 1 Akor . 13 : 4 ) Tikakhala odzicepetsa , anthu ena adzakopeka na kufuna kuphunzila za Yehova . Anzanga anayamba kuniseka , kunizunza , ndi kunitema na zinthu cifukwa codziŵa kuti siningawabwezemo . Onani ndemanga izi zimene oyang’anila dela ena anakamba : “ Pamene nilalikila na abale na alongo okhulupilika amenewa , nimalimbikitsiwa ngako na citsanzo cawo . ” Caciŵili , Mulungu ni “ Atate wathu . ” Ndinali kufunika kupeza nchito yabwino koma ndinalibe mapepala a kusukulu . Ngakhale kuti ndise makolo ogontha , tinalela ana aamuna 7 amene amamva . Pamene nthawi inafika , Yehova anapeleka malangizo omveka kuti asiyanitse alambili okhulupilika ndi apandu . Ni mfundo iti imene tifunika kukumbukila pa nkhani ya kukhala wodziŵika kwa Yehova ? 4 : 8 ) Zonse zimene analenga ndiponso zimene amacita zimaonetsa kuti iye ni wacikondi . Kodi cikhulupililo na cikondi amazichula bwanji m’Malemba ? Nanga ni khalidwe liti lalikulu kwambili pa aŵiliwa ? ( 2 Samueli 12 : 7 - 14 ) Kodi Davide anacita ciani ? Imeneyi ni nthawi yokonzekeletsa maganizo athu kuti timvele nkhani zimene abale adzakamba . Koma anthu ena saikako nzelu ku zimene zicitika . Yakobo 5 : 13 - 15 Komanso tapeza mabwenzi atsopano apamtima . Ndipo pemphani mnzanuyo kucita cimodzi - modzi . Ena amakhumudwa akaona kuti sangapewe kupondelezana kumene kuli m’dzikoli lopanda cilungamo . Koma muziganizila mozama zimene muŵelengazo , ndipo muzidzifunsa mafunso monga awa : ‘ Ni makhalidwe abwanji amene naona mwa munthu amene nikuŵelenga nkhani yake ? Ngakhale n’telo , anthu ena osakhulupilila sagwilizana nazo . 10 : 24 , 25 . * Koma amene acititsa kuti vutoli lipitilize ndi anthu . Njila ina imene Yehova anatetezela anthu ake kale ndiponso masiku ano , ndi kupitila mwa angelo . Nchito yolalikila siiyenela kukhala bizinesi 2 : 15 ) Koma izi sizitanthauza kuti kubala ana n’kumene kungapangitse munthu kudzakhala na moyo wosatha . Yehova watipatsa mwai waukulu wokhala Mboni zake . ( Yes . ( Luka 3 : 21 , 22 ; Yoh . ( Machitidwe 16 : 4 , 5 ) Ici cinali ciyambi cabe . Kuti mudziŵe zambili ponena za kusiyana pakati pa moyo wosafa ndi moyo wosatha , onani Nsanja ya Olonda yacingelezi ya April 1 , 1984 , masamba 30 - 31 . . ( 2 Pet . 2 : 5 ) Kulalikila , kumanga cingalawa , ndiponso kugwilizana ndi anthu a m’banja lake kunacititsa Nowa kuika maganizo ake pa kucita zinthu zabwino zimene zinakondweletsa Mulungu . Umoyo unali conco mpaka pamene zinthu zinasintha . Kupatulapo nkhondo yoyamba ya padziko lonse , pacitika nkhondo zina zoopsa zimene zacotsa mtendele padzikoli . Makolo anu , bwenzi lanu , kapena mnzanu wa m’cikwati angakuthandizeni kucepetsa nkhawa ndi kukhulupilila Yehova . Mlongo Diane wa ku Canada anati : “ Poyamba cinanivuta kukhala kutali na acibanja . ” 32 Kodi Mudziŵa ? Kucita zimenezi kumacititsa kuti anthu ena azikopeka ndi paladaiso wauzimu ameneyu . Lemba la Yohane 19 : 38 limati Yosefe “ anali wophunzila wa Yesu koma wamseli cifukwa anali kuopa Ayuda . ” Anali asanaphunzile kulalikila na Baibo cabe . Anali kudalila buku lakuti The Finished Mystery “ kuwalankhulilako . ” Tingacite ciani kuti tipite patsogolo panthawi imodzi - modzi tithandizenso ophunzila Baibulo kupita patsogolo ? KUCEZA NDI MNZATHU Izi zinatilimbikitsa kuyamba kugwila nawo nchito yolalikila . Tsiku lina , n’namenyedwa pamene n’nali kulalikila . ” Akristu onse oona amafuna kutsatila citsanzo ca M’busa Wamkulu . Iye anali kuweluza milandu m’malo mwa Yehova . — Oweruza 4 : 4 , 5 . Cinaniŵaŵa kwambili , ndipo n’nakhumudwa . ” Iye ali pafupi ndi onse amene amamuitana m’coonadi . ” — Salimo 145 : 18 . 28 “ Mvelani Malangizo Kuti Mukhale Anzelu ” Pokhala Mikayeli mkulu wa angelo , Yesu “ anasemphana maganizo ndi Mdyerekezi ndipo anakangana ” ndi woipayo . ▪ Mudzakhala “ Ufumu wa Ansembe ” 18 : 17 - 25 ) Eliyakimu anatumiwa kuti akakambilane na nthumwizo , koma sanapite yekha . ( Yobu 21 : 7 , 9 ) Koma , Baibo imati : “ Maso [ a Mulungu ] amayang’anitsitsa njila za munthu , ndipo amaona mayendedwe ake onse . Pamene ena mwa ophunzila ake anali kukangana kuti wamkulu ndani , iye anawalangiza mokoma mtima ndipo anawauza citsanzo ca mwana wang’ono pofuna kuwaongolela . 54 : 13 ) Monga mmene Yesu analonjezela , Yehova watidalitsa pali pano pokhala m’banja lokondana la padziko lonse , banja lauzimu , inde banja la abale na alongo . ( Yobu 1 : 1 ) Yobu anafuna kukondweletsa Mulungu panthawi yabwino komanso yovuta . Kodi inu ndinu m’modzi wa iwo ? Ndiyeno n’napemphedwa kuti nikatumikile mu tauni ya Feldbach , kumpoto cakum’mawa kwa mzinda wa Graz . Posacedwa , lonjezo la Mulungu la paradaiso padziko lapansi lidzakwanilitsidwa . Mfumu yoikidwa ndi Mulungu ya Ufumu umenewu ndi Yesu Kristu , amene ali ndi mphamvu yocilitsa odwala . Cifukwa cakuti kukali zaka zambili kuti mbadwa za Abulahamu ziloŵe M’dziko Lolonjezedwa , Melekizedeki , mfumu ya ku Salemu , analinso “ wansembe wa Mulungu Wam’mwambamwamba . ” ( Aheb . Iye ali limodzi ndi atumwi ake anai , Petulo , Andireya , Yakobo , ndi Yohane . Iwo akuchela khutu kwambili pamene Yesu akuwafotokozela za ulosi wocititsa cidwi wokhudza tsogolo . Pambuyo pake , anadziimba mlandu cifukwa ca zimene anacita . N’napeza amayi , atate , abale na alongo anga auzimu , monga mmene Yesu analonjezela . ” — Maliko 10 : 29 , 30 . Kodi kacisi wamkulu wauzimu wa Mulungu n’ciani ? Nanga anakhazikitsidwa liti ? Iye watipatsa Malemba Opatulika ndi mzimu woyela umene umathandiza anthu ake . Kodi tingakonzekele bwanji zocitika zimene zingayambitse mikangano ? Koma ufuluwo supatsa anthu mphamvu yopandukila Mlengi wawo amene anawapatsa moyo . Mwina iye anaganiza kuti , ‘ M’malo moti wina azindiuza kuti cabwino ndi ici , coipa ndi ici , ndizisankha ndekha . ’ Anthu a m’dzikolo amene sanali kulambila Yehova , anasonkhezela Aisiraeli kuyamba kulambila milungu yawo . Zimenezi zionetsa kuti panali zakudya zoculuka kwambili . Yehova amafuna kuti tikhale owolowa manja monga mmene iye alili . Conco , kuti tipewe kudzipatula , tifunika kugwilizana ndi anthu amene amaopa Mulungu ndi kulemekeza miyezo yake . Tasonyeza deti la magazini imene muli nkhani Ndiyeno , anasamukila mu mzinda wa Cleveland , ku Tennessee pamodzi na alongo ena kukatumikila kosoŵa . Cifukwa ca kuona kufunika kwa alaliki a Ufumu , Aleksey amacita upainiya wothandiza akakhala pa holide . Ndiponso Lameki , mbadwa yake ya Kaini , ndiye anali woyamba kudziŵika kuti anakwatila akazi aŵili . Pali anthu ambili amene poyamba anali oopsa monga mimbulu , koma lomba amakhala mwamtendele ndi anzawo . Woyang’anila dela anacezelanso mpingo wao ca posacedwapa . 2 : 3 , 4 ) Yesu anakamba kuti kupewa mtima wodzikonda n’kofunika kwambili pa kulambila kwathu . 6 : 2 - 4 . Mmodzi wa Mboni za Yehova anatumiza uthenga kwa ofalitsa magazini ino pamodzi ndi copeleka . Mu uthenga wake iye anati : “ Kwa zaka zambili , nakhala nikupeleka ndalama yocepa pa Nyumba ya Ufumu . Zipembedzo zambili padziko lapansi zili ndi akacisi opatulika , * ndipo anthu ambili amapita ku akacisi amenewo . Atalalikila m’madela ambili , Yesu ndi atumwi ake anaganiza zopita kwaokha kuti akapume . Mayi wina atakhala na mwana wamwamuna kudziko lacilendo , anafuna kutumiza mwanayo kudziko la kwawo kuti makolo ake akamusungile . Ngakhale kuti panapita zaka kuti Kevin asinthe , iye anasinthadi ndipo anakhala mtumiki wothandiza . N’nali kudzifunsa kuti , ‘ N’cifukwa ciani ? Caciŵili , tiyenela kuyesetsa “ kusunga umodzi wathu mwa mzimuwo . ” Madalitso amene tapeza ine na Maria cifukwa cokhala okhulupilika ni oculuka kuposa amene tinali kuganizila . Tingacite ciani kuti Mulungu atidziŵe ? Aikapo Genesis 3 : 17 - 19 ndi Aroma 5 : 12 . Kodi nchito yolalikila imagwilizana bwanji ndi colinga ca Yehova cokhudza anthu ? Ndiyeno anapitiliza kufotokoza mmene Mulungu amasamalila maluwa akuchile . Iye anati : “ Kodi iye sadzakuvekani kuposa pamenepo , acikhulupililo cocepa inu ? Gulu la Mulungu linapeleka malangizo amenewa kuti ophunzila atsopano azikhazikika bwino m’cikhulupililo . Ndiyeno , anawacenjeza mobweleza - bweleza kuti : “ Khalani maso . ” Tisalole nyimbo za kudziko , mavidiyo , mapulogalamu a pa TV , mabuku , anzathu , aphunzitsi , kapena anthu odzicha akatswili kutsogolela umoyo wathu . — Akol . Moyo wa Inoki unali pangozi . Pokambilana zingakhale bwino kupenda lemba la Maliko 10 : 29 , 30 . ( b ) Kodi makolo ndi ana angakonzekele bwanji mavuto amene angabwele ? SANGALALANI MWA KUCITA ZIMENE MUNGATHE Mu 1914 , ni anthu ocepa amene anali kulambila Yehova . ( Aroma 15 : 4 ) — 3 / 15 , masamba 17 - 18 . Anali kukonda kwambili Yehova , ndipo anadzipeleka ngako pothandiza ena . Ponena za nchito ya Mboni za Yehova , wocita kafukufuku wina anati : “ Colinga cao cacikulu ndi kulalikila ndi kuphunzitsa anthu . ” Tingapindule bwanji ngati tivomeleza ciitano ca Mulungu cakuti tizipemphela kwa iye ? Anthu okhala ku Yerusalemu anali kuzidziŵa bwino mbalame zochedwa namzeze ( ena amati nyamkalema ) , zimene nthawi zambili zimamanga zisa munsi mwa mtenje wa nyumba . Kudzatithandizanso kukhala ndi cimwemwe ndi kupanga zosankha zanzelu podziŵa kuti tidzakhala kwamuyaya . Iye anakamba kuti : “ Aliyense woyang’anitsitsa mkazi mpaka kumulakalaka , wacita naye kale cigololo mumtima mwake . N’kutheka kuti timacita manyazi kuimba nyimbo cifukwa sitidziŵa bwino mmene tingaimbile . Nanga bwanji ngati mnzanu wa m’cikwati , mwana wanu , kapena mnzanu wacotsedwa mumpingo koma inu simukugwilizana nazo ? Ngati io aphunzitsidwa bwino , angasamalile maudindo ambili mumpingo . Iwo amacita mwambo umenewo ngakhale zinthu zivute bwanji . Asanayambe kuvutika , iye anali “ munthu wolemekezeka kwambili pa anthu onse a Kum’mawa . ” “ Zinthu zimene zinali kundisangalatsa , zinali zokhudzana ndi ana a anthu . ” — MIY . Komabe , zoipa zimene anthu amacita sizim’landa cimwemwe . Dziko lopanda asilikali , zida za nkhondo , kapena zipilala zokumbukila zimene zinacitika pa nkhondo . Pelekani citsanzo . ( b ) N’cifukwa ciani anthu amene amapenyelela zamalisece afunika kupempha thandizo mwamsanga ? Pavel anatumikila ku Sakhalin mpaka mu 1995 . ( Danieli 7 : 13 , 14 ) Popeza kuti Mulungu ndiye anasankha Wolamulila wa Ufumu wake , anthu sacita masankho ndiponso sangauthetse . ( Luka 11 : 28 ) Koma koposa zonse , kusinkhasinkha Mau a Yehova tsiku lilionse kudzatithandiza kucita zinthu zimene zimam’lemekeza . Koma kodi Paulo anatanthauza ciani pamene anakamba kuti malemba oyela adzathandiza Timoteyo kupeza ‘ nzelu zomuthandiza kuti akapulumuke ’ ? Taphunzilanso kuti kudzicepetsa n’kofunika kwambili . ” 7 , 8 . ( a ) Ndi nkhani iti imene Akristu ayenela kutengamo mbali ? Kodi pemphelo lingakuthandizeni bwanji kulimbitsa cikhulupililo canu ? Papita zaka 2,000 kucokela pamene Yesu anatifela , koma tikupindulabe ndi dipo lake lelolino . Ciheberi na Cigiriki camakono n’cosiyana ngako na cimene cinaliko panthawi imene Baibo inali kulembedwa . Komabe , vinyo unali kupelekedwa kwa anthu amene anali kuona kuti “ vinyo woŵila ndi umene unali kufunika kugwilitsilidwa nchito . ” Munthu aliyense amene amatsatila citsanzo ca Yesu amafunika kucitila cifundo anthu ena , kuphatikizapo abale ake auzimu . ( Yoh . 13 : 34 , 35 ; 1 Pet . Nafenso , limodzi ndi anthu ena , tikulakalaka kudzavina cifukwa ca cimwemwe m’dziko latsopano la Yehova . — Eks . Maapozi agolide amaoneka okongola , koma amaoneka okongola kwambili akakhala m’mbale ya siliva . Anthu akhala akutsutsana kwa zaka zambili pa nkhani imeneyi . Ndiyeno , anakhala na ciyembekezo ca kumwamba . Aya ni mafunso ofunika ngako , koma adzayankhiwa m’nkhani yotsatila . Mfundoyo imati : “ Aliyense wofika kwa Mulungu ayenela kukhulupilila kuti iye alikodi , ndi kuti amapeleka mphoto kwa anthu omufunafuna ndi mtima wonse . ” Yesu analonjeza gulu lina kuti lidzakhala ndi moyo kumwamba . Tikalonjeza kuti tidzapita , tiyenela kukwanilitsa lonjezo lathu . Ni zitsanzo za m’Malemba ziti zimene zionetsa kuti Yehova angaticitile zinthu zimene sitinali kuyembekezela ? Mfundo imodzi ili pa Miyambo 18 : 13 , imene imati : “ Munthu aliyense woyankhila nkhani asanaimvetsetse n’ngopusa , ndipo amacita manyazi . ” Tiyeni tsopano tikambilane mafanizo atatu mwa mafanizo amenewo ndi kuona zimene tikuphunzilapo . Alisa , mlongo wocokela ku Russia wa zaka za m’ma 30 , anakamba kuti : “ Kutumikila Yehova mwanjila imeneyi kwanithandiza kuona ubwino wonse wa Yehova . ” ( Sal . Kodi Yehova anayamba liti kukhala ndi anthu apadela padziko lapansi ? 14 , 15 . ( a ) Kodi tiyenela kusamala ndi anthu otani ? Tinakwanitsa kupeza thilansipoti yotipeleka ku Wichita , kumene m’bale E . N’ciani cimene Yehova wakhala akucita kuti nchito yolalikila ipite patsogolo masiku ano ? Mwacitsanzo , mzinda wa São Paulo , ku Brazil uli ndi anthu ambili . Koma kunacoka lipoti lakuti kupha anthu kwacepekela ndi 80 pelesenti m’zaka 10 zapita . ( Genesis 1 : 26 ) Iye anapatsa anthu ufulu wodzisankhila zocita , ndipo io angasankhe kum’konda ndi kukhala okhulupilika kwa iye mwa kucita zinthu zoyenela pamaso pake . N’nali na maphunzilo okwana 15 kapena kuposelapo . Mofanana ndi zimenezi , tingakhale ndi zinazake zabwino zimene tifuna kuuza munthu . Monga mmene cilengedwe cionetsela , Yehova mwacikondi anaika malamulo . Ndiyeno , Margaret amene anali katswili wodziŵa kuphika , anakonza zakuti aphike makaloni na chizi monga cakudya colaililana , cakudya cimene adzukulu awo aŵili amacikonda kwambili . Tsiku lina , pamene n’nali kuyenda m’tauni pa motoka yanga yofiila , atsikana aŵili ananibaibitsa . Tikalakwila Yehova , timakhala ndi ngongole kwa iye . N’zoonekelatu kuti Yesu akupitilizabe kuphunzitsa anthu ambili . Ndipo adzapanga dziko lapansi kukhala malo abwino okhalamo anthu . — Ŵelengani Salimo 37 : 11 , 29 ; Yesaya 55 : 11 . Komanso ndinali kupemphela kuti andithandize kudziŵa colinga ca moyo . Conco , atangofika m’dzikolo , anamanga guwa la nsembe pamalo pamene panali kacisi woyambilila , ndipo anayamba kupeleka nsembe kwa Yehova tsiku lililonse . Izak Marais Koma mpaka pano , kulibe ngakhale mmodzi anakhala mboni . MWAMUNA wina wochedwa Eduardo * anati : “ Nditapita kudziko lina ndinapeza nchito yabwino ndipo ndinali kulandila ndalama zambili . Ndipo ngati tiona zinthu moyenela , tingaonetse kuti timakonda abale ndi alongo athu mwa kuwalimbikitsa ndi kuwatonthoza . Mofanana ndi akapolo aŵili oyamba aja , abale ndi alongo odzozedwa akhala akucita khama pa nchito yao yolalikila . Popeleka lonjezo la mu Edeni , Mulungu woona anati : “ Ndidzaika cidani pakati pa iwe [ Satana ] ndi mkaziyo , ndi pakati pa mbeu yako ndi mbeu yake . ” 1 : 23 ) Kukula kumeneku kunali kopindulitsa cifukwa cakuti Yesu anakamba kuti ‘ mbalame zam’mlengalenga zinabwela kudzapeza malo okhala munthambi zake . ’ Kumbukilani kuti Heledai , Tobiya , ndi Yedaya anapeleka golide na siliva amene Zekariya anapangila cisoti cacifumu . Dzifunseni kuti , ‘ Kodi nimayesetsa kucita zinthu zokondweletsa Yehova , kuteteza kulambila koona , ndi kuteteza anthu a Mulungu ku zinthu zimene zingawaononge mwauzimu ? ’ Ganizilani za Asa . Cikondi ceniceni “ sicisunga zifukwa , ” koma ‘ cimakwilila macimo oculuka . ’ N’nawakonzekeletsa mlanduwo ndi kuwafunsa mafunso mwa kuyeselela kukhala loya . Sadana ndi cipembedzo canga , ndipo amandisangalatsa kuposa abale ena . ” Tingacite ciani kuti tione phindu la cilango cocokela kwa Mulungu ? Conco , tiyeni ‘ tizipemphela mosalekeza . ’ 10 : 6 - 11 ) Panopa tili ku mapeto enieni a “ masiku otsiliza ” ndipo pokhala atumiki a Mulungu , tatsala pang’ono kuloŵa m’dziko latsopano lolungama . ( 2 Tim . 3 : 1 ; 2 Pet . Iye wayeletsa gulu la anthu odziŵika ndi dzina la Yehova . Ndipo kumakhala ndi zotulukapo zotani ? KUKHALA wokhulupilika ndi kusatengako mbali mundale ndi nkhani imene imakhudza Akristu nthawi zonse ngakhale pamene kulibe nkhondo . Mwacitsanzo , tiyenela kupemphelela abale , alongo , ndiponso ana amene ali m’ndende m’dziko la Eritrea . Abale athu awa : M’bale Paulos Eyassu , Isaac Mogos , ndi Negede Teklemariam ali m’ndende m’dzikoli ndipo akhalamo kwa zaka zoposa 20 . Zimenezi zimamucititsa kuzindikila anthu , zinthu ndiponso zinthu zina zimene zikucitika . M’caputala 24 ca buku la Mateyu , Yesu anafotokoza za “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” Kapepala kalikonse kamatilimbikitsa kuŵelenga lemba loyenelela . Nchito imeneyi yathandiza anthu ambili kutuluka m’cipembedzo conama ndi kumasulidwa ku ulamulilo wa Satana . “ Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha ” ? — Yohane 3 : 16 . A Zimba : N’zoona . Makolo angaphunzile kupeleka cilango mwacikondi kwa ana awo . Ndiyeno Yesu adzabwezela Ufumu kwa Atate wake . Dziko lapansi likondwele , ndipo zilumba zambili zisangalale , ” ndi oona . — Sal . Ndi mphatso yabwino iti imene makolo angapatse ana ao ? Nanga mwana ayenela kucita ciani ndi mphatsoyi ? Oyang’anila dela ena ali na nkhawa cifukwa nthawi zambili amapeza acicepele a zaka pafupi - fupi 20 kapena kuposelapo , amene sanabatizikebe olo kuti anakulila m’banja la Mboni . Iwo sanafune kusintha zocita zao ndi maganizo ao . Ganizilani cabe cimwemwe cimene iye anakhala naco ! ZINENELO : Baibulo lonse kapena mbali yake , lamasulilidwa m’zinenelo zoposa 2,500 Iye analemba mosapita mbali kuti ana acikristu , adzukulu , ndi acibale ena ndi amene anali ndi udindo waukulu wosamalila akazi amasiye okalamba m’banja lao . Tiyeni tikambilane za mabwenzi ena atatu a Yehova amene amachulidwa m’Baibulo . ( 1 ) Rute , mkazi wamasiye wokhulupilika wa ku Mowabu , ( 2 ) Hezekiya , Mfumu yokhulupilika ya Yuda , ndi ( 3 ) Mariya , mai wodzicepetsa wa Yesu . Tifunika kumayakonda na kuyalemekeza . Ndipo zimenezi n’zomveka makamaka tikaŵelenga ulosiwu wonse . ( Oweruza 5 : 30 ) Mau akuti “ mkazi ” pa lemba limeneli akutanthauza “ mimba . ” Ambili angayankhe kuti inde , cinacake m’thupi mwathu — cochedwa mzimu — sicimafa . 25 : 19 . Iye anaona kuti anthu amenewo anali na mtima wofuna kucita zabwino . Mlongo Matilda , amene watumikila monga mpainiya kwa zaka 20 , anati : “ Zimanikondweletsa kudziŵa kuti Yehova adzatidalitsa cifukwa ca nchito imene timagwila modzipeleka . ” Zofalitsa zimene amalembela acinyamata zingawathandize kulimbitsa ubwenzi wao ndi Yehova . ( Ezek . 37 : 21 , 22 ) Apa Aisiraeli anayambanso kutumikila Yehova mogwilizana . Ndiyeno anabatizika . Mau a Mulungu amasintha anthu amene amawaŵelenga ndi kukhulupilila malonjezo amoyo a Yehova . Amuna ndi akazi angalole Yehova kutsogolela banja lao mwa kutsatila malangizo ake acikondi . Ine ndi Susan tinakhala ndi ana aŵili aamuna . Maina ao ndi Jesse ndi Paul . Iye anakamba kuti io anagwilitsila nchito Baibulo ndipo anam’thandiza kuti aleke kuganizila kwambili zoipa zimene ena anakamba ndi kuyamba kuganizila kwambili za Yehova . ( 1 Sam . 25 : 10 - 13 ; 2 Sam . 11 : 2 - 4 ) Ngakhale n’conco , tingaphunzile mfundo zofunika kwa Davide . Tingapemphele kwa Yehova nthawi iliyonse . Pa nthawiyo , iwo anali na zaka za m’ma 50 . Didier anati : “ Tinacitapo upainiya tili acinyamata . Kuwonjezela apo , Yobu anadziŵa makhalidwe a Mulungu osaoneka mwa kuyang’ana cilengedwe cake . Tidzaphunzilanso mmene tingaonetsele kuti ndife oyela m’makhalidwe athu onse . 12 - 14 . ( a ) Kodi Eliya anavutika ndi maganizo ofooketsa ati ? Iye anali kukonda anthu , ndipo anali kuona miyoyo yawo kukhala yamtengo wapatali . ( 1 Akor . Kodi tingakhale bwanji mogwilizana ndi pempho lakuti cifunilo ca Mulungu cicitike padziko lapansi ? Mwina Mkristu amene wakukhumudwitsani ali ndi maudindo ambili mumpingo ndipo ena amamuona kuti ndi Mkristu wabwino kwambili . ( b ) Kodi kholo lililonse lacikhristu limafuna kupeza cimwemwe cotani ? ( Genesis 26 : 8 ; 1 Samueli 1 : 5 , 8 ; 1 Petulo 3 : 5 , 6 ) Mwamuna ndi mkazi akamacita zimenezi , amakhala ogwilizana ndipo amayandikila Yehova kwambili . — Ŵelengani Mlaliki 4 : 12 . Pofuna kudziteteza , Petulo anakana Yesu katatu . — Mat . Tingaphunzile ciani kwa Yesu pa nkhani ya kupeleka cilango moyenelela na kuphunzitsa mogwila mtima ? Masiku ano , sinilephelanso kugona usiku cifukwa coopa zamtsogolo kapena imfa . Kodi mumatsutsidwa kapena kuzunzidwa ndi anthu ena ? Conco , kuyambila kale otsatila a Yesu apitilizabe kukhala chelu . Kodi zoona anthu adzaononga dziko lapansi kothelatu ? Masomphenya amenewa amatithandiza kudziŵa zambili za mmene kumwamba kulili . 3 : 11 - 15 ) Masiku ano , akulu angapeleke nkhani yocenjeza mpingo cifukwa ca munthu wina amene akupitiliza kucita zinthu zobweletsa citonzo pa mpingo , monga kukhala pacibwenzi na munthu amene si Mboni . ( 1 Akor . Pokhala anthu wamba , sitingadzipulumutse tekha kapena kupulumutsa wina . Sikuti iye ali cabe ndi cikondi , koma iye ndiye cikondi . 6 : 2 ) Kodi Baibulo , zofalitsa zathu ndi misonkhano ya mpingo imakuthandizani kudziŵa kuti Mulungu amakusamalilani ? Koma Yesu anaukitsidwa ndi thupi lauzimu limene silingafe . ( Miy . 18 : 13 ) Coyamba tiyenela kuwaonetsa kuti timawadela nkhawa anthu amene amaziona kuti ndi ‘ osalemekezeka ’ cifukwa ca zimene amakumana nazo . ( 1 Akor . Ganizilani mmene nchito yanu imapindulitsila ena . Mu ulamulilo wa Yesu Khristu , “ padzakhala mtendele woculuka kwa nthawi yonse pamene mwezi udzakhalepo , ” kutanthauza kwamuyaya . — Salimo 72 : 7 . Yehova anaona nchito zabwino za Sifira ndi Puwa ndipo anawadalitsa mwa kuwapatsa ana aoao . Kuti zinthu zonsezi zicitike , panafunika kutenga nthawi . — Ezekieli 37 : 7 - 10 , 14 . Kodi zimene wacita zionetsa kuti iye ali ndi vuto linalake ? ’ ( Miy . 12 : 18 ) Koma amationa kuti ndise ofunika , ndipo amayang’ana kwambili pa zabwino zimene timacita . ( Yes . Conco , tiyeni tipitilize kukumbukila ‘ nchito zacikhulupililo ndi zacikondi ’ za atumiki anthawi zonse . — 1 Ates . Pali mphatso inanso imene inawathandiza . Aisiraeli anakumana ndi mavuto aakulu cifukwa cogwilizana ndi anthu oipa . 23 : 10 . Anauza ophunzila ake kuti : “ Ine sananditumize kwa wina aliyense koma kwa nkhosa zotayika za nyumba ya Isiraeli . ” ( Mat . 7 : 12 ) Kodi anthu amene akukila mu mpingo mwanu mungawaitaneko kunyumba kwanu kuti mudzacite nawo kulambila kwa pabanja kapena kutamba nawo pulogilamu ya pa mwezi ya JW Broadcasting ? Ndipo mu 1993 , abale mu Kyrgyzstan anacita msonkhano wacigawo woyamba mu sitediyamu ya Spartak mu mzinda wa Bishkek . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Aliyense asamangodzifunila zopindulitsa iye yekha basi , koma zopindulitsanso wina . ” — 1 Akorinto 10 : 24 . Ndipo mumafunanso ana anu kuti azidzimva monga wamasalimo amene anati : “ Ndimakondwela ndi kucita cifunilo canu , inu Mulungu wanga , ndipo cilamulo canu cili mumtima mwanga . ” Yesu ndi wokoma mtima kwambili . A Daka : Mmm . Conco , iye analemba mau oonetsa liu leni - leni m’zilembo zakuda kwambili , koma aphatikila a kumbuyo ndi a kutsogolo anawalemba m’zilembo za nthawi zonse ( zosada kwambili ) . Koma kodi ubongo umenewu unapangiwa kuti uziphunzila zinthu na kudziŵa maluso basi pambuyo pake n’kufa ? Ngakhale n’conco , mukadwala , Yehova adzakulimbikitsani ndi kukucilikizani monga mmene anacitila kwa atumiki ake akale . Tinali kukhala umoyo wosalila zambili kumidzi . Kunalibe malaiti , tinali kugona pamphasa , ndipo pa maulendo tinali kuseŵenzetsa ngolo yokokedwa na hosi . Iye amafuna kulepheletsa nchito yathu yolalikila uthenga wa Ufumu , ndipo amacita zimenezi mwa kugwilitsila nchito njila zooneka ndi zobisika . N’zolimbikitsa kudziŵa kuti Yehova amatha kulamulila mphamvu zacilengedwe . Kupanduka kwa Adamu na Hava kunabweletsa mavuto aakulu m’banja mwawo , komanso m’mabanja onse am’tsogolo . Gumbwa imang’ambika mosavuta , imasintha maonekedwe , ndipo imawonongeka . Kodi zingacitike bwanji kuti tilole ena kutipangila zosankha ? N’ciani cingathandize acicepele kuti asalole zinthu zina kuwatangwanitsa pamene akuyesetsa kukwanilitsa zolinga zawo ? ( Agal . 5 : 22 , 23 ) Mofanana ndi cipatso ceni - ceni , cikhulupililo cimatenga nthawi kuti cikule . Ngakhale kuti mumakhala kutali ndi makolo anu mudzafunikila kuona zimene amafunikila tsiku ndi tsiku . Mpaka lomba , John akali na cipsela ku cala cake ca kudzanja lamanja cimene anadziceka zaka 60 zapitazo . Tifunika kusamala kuti cikondi cathu pa Khristu cisazilale ndiponso kuti tisalole zinthu zina kutilepheletsa kuika zinthu za Ufumu patsogolo . Ndiyeno , muzicita zinthu mogwilizana ndi mapemphelo anu . Mosakaikila pamene anali kukambilana ndi mngelo , Gidiyoni anali kuona kuti Yehova ndi weni - weni . Pamene ndinapita muulaliki ndi apainiya ena ndinaona kuti anthu ambili anali kufunitsitsa kuphunzila coonadi . Mwina inunso mumamvela cimodzi - modzi mukaganizila mavuto ambili - mbili amene Satana wacititsa . Onani nkhani ya Asa yamutu wakuti , “ Mudzapeza Mphoto Cifukwa ca Nchito Yanu , ” mu Nsanja ya Olonda ya August 15 , 2012 . Lemba la Zefaniya 1 : 14 limati : “ Tsiku lalikulu la Yehova lili pafupi . N’cifukwa ciani tifunika kuzindikila kuti kupanga zosankha ni mbali ya umoyo ? Posakhalitsa , na ine n’nakhutila kuti zimene n’nali kuphunzila ni coonadi . “ MULUNGU ALIBE TSANKHO ” Baibulo limati : “ Mulungu alibe tsankho . Iye amalandila munthu wocokela mu mtundu uliwonse , amene amamuopa ndi kucita cilungamo . ” Popeza tikali m’dziko la Satana , tidzapitilizabe kukumana ndi mavuto . 15 : 11 - 13 ) Kuwonjezela apo , Asa analimbikitsa anthu “ kuti afunefune Yehova Mulungu . . . ndi kutsatila cilamulo . ” YANKHO : Iyai . ( b ) Ndipo anafotokozanso ciani ? Angelo ena anagwilizana na Satana , ndipo anayamba kuchedwa ziwanda . ( Aheb . 2 : 14 ) Conco , mkazi amene akubeleka mbeu ayenelanso kukhala colengedwa cauzimu . TSAMBA 3 • NYIMBO : 5 , 60 34 : 18 . * Iye anavomela kuti tiyambenso kuphunzila koma tinakumana ndi mavuto aŵili . Yehova “ anatsegulila anthu a mitundu ina khomo loloŵela m’cikhulupililo . ” Ndiyeno mu 1939 , Nkhondo Yaciŵili ya Dziko Lonse itakula ku Europe , m’mudzi wathu munacitika zinthu zimene zinatidabwitsa ngako . Mwacitsanzo : M’bale amene watumikila monga mpainiya wanthawi zonse , mpainiya wapadela , mmishonale , ndipo pa nthawi ino akutumikila pa Beteli ku dziko lina anati : “ Ndaona kuti kuyamba utumiki wanthawi zonse ndi cosankha cabwino koposa cimene ndinapanga . Nanga n’cifukwa ciani panafunika zimasulilo zina za Baibo ? ( Yoh . 8 : 31 , 32 ) Malinga n’zimene Yesu anakamba , pali zinthu ziŵili zimene tifunika kucita kuti tidzapeze ufulu weni - weni : Coyamba , kuphunzila coonadi cimene iye anaphunzitsa , ndipo caciŵili , kukhala wophunzila wake . Kodi cifukwa cikulu cimene tiyenela kucilikizila ulamulilo wa Yehova n’citi ? Iye anati : “ Mitundu yonse isonkhanitsidwe pamalo amodzi , ndipo mitundu ya anthu ikhale pamodzi . Mu 1978 , tinakhala a Mboni za Yehova . Umbeta suyenela kucita kukhala mtolo iyai . Padziko lonse , anthu a Yehova amakamba zitundu zosiyana - siyana . Komabe , Baibo imaonetsa kuti ngakhale acicepele angamvetse coonadi ca m’Baibo na kuyamba kucikonda . Ndiponso , pamene anauzidwa kuti wacimwa , iye anavomeleza kulakwa kwake ndipo anacilikiza ziweluzo za Yehova . ( Eks . 32 : 26 ; Num . Mwana wamkazi woyamba m’banjali , dzina lake Livija , anayamba upainiya wa nthawi zonse atangotsiliza maphunzilo a ku sekondale . Ndiyeno , mofanana ndi mtumwi Paulo , tingaime pamaso pa Mulungu ndi kunena kuti “ sitinayambe talankhulapo mau okuyamikilani mwacinyengo , ( monga mukudziŵila ) , kapena kucita zaciphamaso cifukwa ca kusilila kwa nsanje . ” — 1 Ates . Zinthu zinanso zogwilitsa mwala zinatsatilapo . Tingaonetse bwanji mzimu woceleza kwa ena ? Cifukwa cakuti m’caka ca 33 C.E . , Yehova anakana mtundu wa Aisiraeli ndi kusankha mpingo wa Akristu kukhala anthu ake . Mungathandizeko abale ndi alongo anu Conco , tiyeni tikambitsilane nkhani yocititsa cidwi ndi kuona zimene tiphunzilapo . 8 “ Ine Ndili Ndi Ciyembekezo mwa Mulungu ” Kodi ndi zinthu ziti zimene ndiyenela kucita kuti ndikhale mlaliki wogwila mtima wa uthenga wabwino ? ’ Pamene n’nali wacicepele , m’dziko lathu munayamba nkhondo . Nkhunda kapena njiŵa zinali nsembe zimene anthu osauka anali kupeleka . Ngakhale n’conco , mitengo ya mbalame zimenezi anaikweza kwambili . ( Lev . Baibulo limati : “ Maso a Yehova akuyendayenda padziko lonse lapansi kuti aonetse mphamvu zake kwa anthu amene mtima wao uli wathunthu kwa iye . ” M’nkhani ino , tidzakambilana za khalidwe la cifundo , limene limatanthauza kukhudzika na mavuto a munthu wina ndi kufuna kumuthandiza . Ngati munthu si wodzicepetsa ndipo afuna kukhala ndi ulamulilo , cimakhala covuta kuti akhalebe wokhulupilika kwa Mulungu . Yosefe sanakhulupilile kuti abale ake enieni anatsala pang’ono kumupha ndipo anamugulitsa kuti akakhale kapolo . “ Conco ngati wabweletsa mphatso yako paguwa lansembe , ndipo uli pomwepo wakumbukila kuti m’bale wako ali nawe cifukwa , siya mphatso yako patsogolo pa guwa lansembe pomwepo . Tulo ndi mkhalidwe wosadziŵa ciliconse ndipo munthu amene ali mu mkhalidwe umenewu samamva kupweteka . Ndipo citsanzo cathu cabwino ndiye cida camphamvu kwambili cimene tili naco , cifukwa nthawi zonse amaona mmene timacitila zinthu . Ngakhale kuti mwamuna wake anali kum’konda , Hana sanali kubeleka . Anthu ena amapeleka mphatso pa masiku a kubadwa ndi pa zikondwelelo za pa maholide . Anthu ena amati zimenezi zimangosonyeza mmene ubongo wathu umagwilila nchito . * Usiku wina , iwo analota maloto odabwitsa . Iye anati : “ Nthawi zonse ndimayamikila Yehova cifukwa ca ubale wa padziko lonse , popeza ionso ndi banja langa . Iye sanasankhe ngakhale umoyo wa Aiguputo wamba , koma anasankha kukhala pamodzi ndi akapolo . Ganizilani malangizo amene Yesu anapatsa ophunzila ake 70 pamene anawatuma aŵili - aŵili kuti akalalikile . Iye anawauza kuti : “ Mukafika panyumba , coyamba muzinena kuti , ‘ Mtendele ukhale panyumba pano . ’ ( Eks . 4 : 14 - 16 ) Ali pafupi kufa , Mose anali wotsimikiza kuti Mulungu amathandiza atumiki ake kukwanilitsa utumiki uliwonse . Iye anali kudalila Yehova kwambili cakuti anauuza Yoswa kuti : “ Yehova ndi amene akuyenda patsogolo panu . Kodi mungakonzekele bwanji mau amene mudzakamba ? Ngati akanalephela kucita zimenezo , sembe anthu ambili anafa . — Ezek . Mu 1870 , gulu locepa la anthu mumzinda wa Pittsburgh ( Allegheny ) ku Pennsylvania , U.S.A , linayamba kufufuza Malemba . Kodi munthu amene mwafikila wakufotokozelani mmene adzakupimilani ndi mmene mankhwalawo amagwilila nchito ? N’cifukwa ciani kuŵelenga Baibulo yonse n’kofunika ? Nanga kusamba kumene ana a Aroni anali kucita kumaimila ciani ? Buku la Mau ake Yehova limationetsa cifukwa cake anthu ake afunika kukhala ogwilizana . 24 : 45 ) Kodi inu panokha mwaona kuti Yehova amakupatsani malangizo mwamsanga ? Kodi Yesu anagwilitsila nchito mphamvu zake zozizwitsa pothandiza ndani ? N’kutheka kuti munapanga masinthidwe aakulu musanabatizidwe . Mwacitsanzo , ngati timagwilizana ndi anthu amene amakonda ciwelewele , tingayambe kulakalaka kucita ciwelewele . Mboni za Yehova zikukuitanani pamodzi ndi banja lanu kuti mudzamvetsele nkhani imene idzafotokoza cifukwa cake imfa ya Yesu ndi yofunika kwambili ndiponso mmene mungapindulile ndi imfa yake . Sitikaikila kuti Ufumuwo udzathetsa mavuto a mtundu wa anthu . Kodi mumaopa kuti mungadzacitilidwe nkhanza mtsogolo ? ( Afilipi 1 : 10 ; 3 : 8 , 13 , 14 ) Paulo analibe mkazi . Zimenezi zinapangitsa kuti iye ‘ atumikile Ambuye nthawi zonse popanda cododometsa . ’ — 1 Akorinto 7 : 32 - 35 . Mokondwela , abale na alongo a m’kagulu ka ulaliki acoka pa Nyumba ya Ufumu kupita muulaliki ku Lusaka , muno mu Zambia . Conco , Yesu ali ku dzanja lamanja la Atate wake kumwamba , anayamba kuona kuti m’dzina lake anthu ambili anayamba kulapa ndi kukhulupilila kuti iye ndiye njila ya Yehova yopulumutsila anthu . — Mac . 2 : 5 , 11 , 37 - 41 . Tinali kusamalila banja lathu . Kumeneko ndinaphunzila maluso ambili a kavinidwe kucokela kwa aphunzitsi apamwamba . Akristu onse angathe kumvetsa nkhaniyi , kuikumbukila , kuigwilitsila nchito pa umoyo wao ndi kulimbitsa cikhulupililo cao . Nanga ndani ena amene analengedwa monga “ ana ” a Mulungu ? Ganizilaninso za makalata amene atumwi anatumiza ku mipingo m’nthawi ya atumwi . ( Akolose 1 : 23 ) Kodi tiyenela kuyembekezela kuti Mulungu adzatiyankha tikapempha cikhulupililo coonjezeleka ? Komabe , njila imene Yehova amalamulila anthu ndi imene imatipangitsa kumuyandikila . Komabe , ngati sitisonkhela nkhuni , motowo ukhoza kuzima ndi kukhala phulusa . Yehova amatithandiza kukhala ogwilizana kudzela m’misonkhano yacikristu . Baibulo lingatithandize kuona nchito moyenela . Komabe , popemphela kwa Mulungu , sitiyenela kupempha cabe zinthu zaumwini yayi . Nkhani 7 zimenezi , zifotokoza mfundo zimene kwa nthawi yaitali zakhala zothandiza maningi kuti munthu akhale wacimwemwe . N’cifukwa ciani Yosiya anaphedwa ? Ena amaphunzila Baibulo pa foni , pakompyuta kapena pa cipangizo ciliconse cokhala ndi intaneti . Pa lemba la 1 Timoteyo 3 : 1 - 7 , pali ziyeneletso zosiyanasiyana za akulu zokwanila 16 . Ine n’nali mmodzi wa abale amene anaitanidwa . ‘ Ine ndidzalankhula mwaukali wanga woyaka moto komanso nditakwiya kwambili . ’ ” Cifukwa cakuti io sanali kudya “ cakudya cotafuna . ” ( a ) Kodi lemba la Yohane 15 : 8 limafotokoza cifukwa citi cimene tiyenela kugwilila nchito yolalikila ? Kodi mpingo ukanam’thandiza bwanji ? KULIMBITSANSO BANJA NDI UMOYO WA KUUZIMU Kodi Adamu anafunika kupanga cosankha canji ? Nanga zotulukapo zake zinali zotani ? Ndi mfundo ziti zili m’nkhani ino zimene mudzafuna kugwilitsila nchito ? ▪ Gwilitsilani Nchito Mau a Mulungu Ndi Amoyo ‘ Anapitiliza kulabadila zimene atumwi anali kuphunzitsa . Iwo anali kugaŵana zinthu ’ [ ‘ kusonkhana pamodzi . ’ Mwacitsanzo , mu March 2011 , civomezi ndi tsunami zinaononga matauni ambili kum’maŵa kwa dziko la Japan . Ndipo angathe kudzipangila zosankha , monga kutumikila Yehova ndi kumumvela . Kuwonjezela pa kupeleka mphatso za ndalama kapena zinthu zina zamtengo wapatali , pali njila zinanso zopelekela zinthu zothandiza pa nchito ya Ufumu padziko lonse . M’BALE wina dzina lake Julian anati : “ Pamene ndinamva cilengezo cakuti mwana wanga wamwamuna wacotsedwa mumpingo , ndinaona monga dziko landicepela ndipo zonse zathela pamenepo . 12 , 13 . ( a ) Kodi Yehosafati anacita ciani atakumana ndi vuto loopsa ? Kuyambila kale , Mboni za Yehova zakhala zikufotokoza umboni wa m’Malemba woonetsa kuti kucokela mu 1914 , takhala tili m’nthawi ya “ kukhalapo ” kwa Yesu . “ Kuyaka [ kwa cikondi ] kuli ngati kuyaka kwa moto . Tingakhale bwanji adongosolo molingana na Buku la Mau a Mulungu ? Kugwilizana ndi anthu oipa kumaononga makhalidwe abwino . ” — 1 Akor . Coyamba , Don anafunsa Peter kuti akambe ngati adziŵa kuti Mulungu ali na dzina . Ndiyeno , anam’pempha kuti adziŵelengele yekha m’Baibo pa Salimo 83 : 18 . 4 : 29 - 31 ; 7 : 8 - 13 . Kevin anakamba kuti kulamulila mkwiyo wake kunali kovuta kwambili kuposa kusintha zizolowezi zoipa zimene anali nazo asabatizidwe.Koma anakwanitsa kusintha cifukwa ca thandizo la Yehova ndiponso cifukwa coŵelenga Baibulo mwakhama . Amene sanamvele Yehova anali kukana kutsogoleledwa na mzimu woyela wa Mulungu , angelo ake , ndi Mau ake . Iye anawauza kuti : “ Mudzakhala mboni zanga mu Yerusalemu , ku Yudeya konse ndi ku Samariya , mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ” ( Mac . ( a ) Kodi Hana analonjeza ciani , ndipo n’cifukwa ciani ? Tangoganizilani zimene Mfumu Mesiya wacita mkati mwa zaka 100 zoyambilila za ulamulilo wake . Kodi fanizoli lindiphunzitsa ciani ponena za Yehova ndi Yesu ? Cikumbumtima caconco cikhoza kutithandiza kupanga zosankha mwanzelu . Zimenezi zimaonekela ndi mmene Yehova anacitila ndi mtundu wa Aisiraeli . Mpake kuti Yesu anali wosangalala . Ndipo , filimu yozikidwa pa Baibulo inali ndi zithunzi zokongola za mitundumitundu , osimba ogwila mtima , ndi tunyimbo twabwino . Ndipo openyelela anaphunzila zinthu zokhudza cilengedwe , mbili ya anthu , mpaka kudzafika ku mapeto a Ulamulilo wa Yesu Kristu wa Zaka 1000 . — Chiv . Koma pang’onopang’ono ndinakwanitsa kuthetsa mantha . Ndipo Yehova amene ali pampando wacifumu anati : “ Taonani ! Mwina anaganiza kuti , ‘ Kodi ndi kwanzelu kuti ndipitenso ku Iguputo ndi kukakwiitsanso mfumu ? ’ N’ciani cionetsa kuti gulu la Mulungu ndi lofunitsitsa kuthandiza anthu onse mwa kuuzimu ? Kucokela panthawiyo , ndimayesetsa kukumbukila cikondi canga ca poyamba kwa Yehova makamaka ndikakumana ndi ziyeso kapena mavuto ena . N’cifukwa ciani Baibulo limayelekezela lilime ndi moto ? Koma ngakhale pali pano ife timapeza madalitso . Ngakhale kuti mbalame ni zocepa thupi , zimadya kwambili zipatso , mbewu , tudoyo kapena nyongolotsi . Polankhula mmalo mwa Mulungu , mngeloyo anatsimikizila Gidiyoni kuti Yehova adzamuthandizadi . Usiku ulionse nikayamba kuvutika maganizo , na nkhawa zikanipanikiza , n’nali kum’condelela Yehova m’pemphelo . Antonio anali paciopsezo cacikulu cokhudza zaciwelewele . 13 , 14 . ( a ) N’cifukwa ciani tifunika kuyesetsa kupatsa moni alendo amene asonkhana nafe ? Mwacitsanzo , m’Baibulo muli lamulo loletsa oweluza kulandila ziphuphu poweluza milandu , ndipo lamulo limeneli likuonetsa kuti anthu anali kucita ziphuphu zaka zoposa 3,500 zapitazo . 20 : 24 ) Cimeneci cinalidi colakwa cacikulu ! Ndipo ngati , tikudwala timafuna kucita ciliconse cimene cingatithandize kuti ticile ndi kukhala ndi moyo wautali . Tsopano iye akutumikila monga mpainiya ku St . pa webusaiti yathu , mungazigwilitsile nchito pa phunzilo lanu laumwini kuti mulimbitse cikhulupililo canu . Mukamaŵelenga ndi kuphunzila Mau a Mulungu nthawi zonse , muziganizila mmene mawuwo akukukhudzilani ndiponso mmene mungawagwilitsile nchito pa umoyo wanu . Mukatelo , ndiye kuti mukulola Yehova kukamba nanu kupyolela m’Mau ake . Ndinali kusangalala kwambili pa nthawi imene tinali kudyela pamodzi . ( a ) Kodi kudzicepetsa kudzatithandiza kucita ciani tikalandila udindo watsopano ? Pasanapite nthawi yaitali , n’nalandila ciitano cokayamba utumiki wa pa Beteli ku Brooklyn pa September 19 , 1955 . Apa n’kuti nili na zaka 17 . Mtumwi Paulo atafotokoza za anthu a makhalidwe oipa osiyana - siyana amene sadzaloŵa mu Ufumu wa Mulungu , ananenanso kuti : “ Ena mwa inu munali otelo . ” ( Genesis 2 : 16 , 17 ) Ngati Adamu sanacimwe mwa kusamvela Mulungu , akanakhala ndi moyo kosatha . ( Aroma 5 : 12 ) Palibe munthu wopanda ungwilo amene angapeleke dipo kwa Mulungu kuti apulumutse moyo wake kapena wa anthu ena . ( Sal . Baibo imati : “ Mwa cikhulupililo , Sara nayenso analandila mphamvu yokhala ndi pakati ngakhale kuti anali atapitilila zaka zobeleka , cifukwa anaona kuti wolonjezayo ndi wokhulupilika . ” Pamene Solomo anali kubwelela ku Yerusalemu , iye anapitila limodzi ndi mtsikanayo , ndipo m’busa wacinyamata anatsatila mtsikanayo . Akolose 1 : 9 , 10 Pa nthawi imeneyo , ndinali kutonthozedwa kwambili pamene ndinali kuŵelenga za Yehova akukhululukila Mfumu Davide atacita macimo akuluakulu . — 2 Samueli 11 : 1 – 12 : 13 . Pofotokoza mmene anamvela pokamba nkhaniyo , iye anati : “ Cifukwa ca mantha , nkhongono zanga zinali kugundana , manja anga anali kunjenjemela , ndipo mano anga anali kulumana . Tsiku lina Adel amene ndinali kugwila naye nchito anandiimitsa n’kundifunsa cifukwa cimene ndinali kuonekela wacisoni . Satana anauza Hava kuti Mulungu anali kunama , ndi kuti ngati sadzamvela Mulungu sadzafa koma adzafanana naye . Makina ena atsopano amene apangidwa pa zaka 200 zapitazi athandiza anthu a Yehova pa nchito yao yolalikila uthenga wabwino . M’NKHANI yapita , tinaphunzila mmene Akhiristu okhulupilika analoŵela mu ukapolo wa m’Babulo . N’ciani cingatithandize kukhalabe acifundo ndi oganizila ena ? Zimene ndamanga , ndikuzigwetsa , ndipo zimene ndabzala , ndikuzizula . Ndicita zimenezi m’dziko lonse . N’ciani cinawathandiza kukhalabe ndi cimwemwe ndiponso olimba mtima ? — Ŵelengani Luka 10 : 1 , 17 - 21 . Conco , n’nayamba kudzifunsa kuti : ‘ N’cifukwa ciani tili na moyo ? Katswili wina anati : “ Iyi si nthawi yabwino yopanga zosankha . ” Pofotokoza za kukhalapo kwake kosaoneka ndi mapeto a nthawi ino , Yesu anati : “ Kudzakhala cisautso cacikulu cimene sicinacitikepo kucokela pa ciyambi ca dziko mpaka tsopano , ndipo sicidzacitikanso . ” Iwo anamuyesa pa nkhani ya kupeleka msonkho wa dinari imodzi , umene munthu aliyense wolamulidwa na Ufumu wa Roma anali kufunika kupeleka . Koma pamene Davide ndi anchito ake anapempha cakudya kwa Nabala , iye ‘ anaŵalalatila ’ ndipo sanawapatse kalikonse . Aisraeli a m’nthawi ya Yeremiya sanali kudziŵa tanthauzo la zimene zinali kucitika m’nthawi yawo . Ambili amakhulupilila kuti helo ndi malo ozunzilako anthu oipa . ( Miyambo 15 : 23 ) Lembali lionetsa kuti nthawi imene tingakambile mau ena ake ni yofunika ngako . Kodi Yehova amateteza bwanji anthu amene amamukonda ndi kumumvela ? Ine ndi anzanga atatu tikayamba kuimba nyimbo mokweza , iwo anali kutitsatila bwino - bwino . Eee ! Kodi Yehova anaonetsa bwanji kuti amakonda cilungamo ? Nanga zimenezi ziyenela kuti zinawatonthoza bwanji acibululu a Naboti na mabwenzi ake ? Koma zimenezo n’zosatheka ku maiko ena . N’ciani cionetsa kuti n’zotheka anthu opanda ungwilo kuonetsa cikondi copanda dyela ? Yelekezani kuti mukumuona akuoneka wododoma pamene akuti : “ Yehova ananditseka kuti ndisabeleke ana . ” Motelo , n’kutheka kuti Yesu anapita ku Yerusalemu ndi kuimilila pamwamba penipeni pa kacisi . Koma kwa ife nkhaniyi ndi yofunika kwambili . Iwo adzaona kuti ngakhale anthu amene akhala m’banja kwa zaka zambili , amafunika kusonyezana cikondi ndi kugwilizana . — Tito 2 : 3 - 7 . Kodi mungakonde kudzakhala m’dziko laconco ? Mu October caka cimeneco , M’bale Russell anakambanso nkhani m’matauni ena , ndipo kumeneko kunalinso anthu ambili omvetsela . Pamene Satana akuyesa kulepheletsa colinga ca Mulungu , amacitanso zinthu zina zoonetsa kuti ndi wankhanza . 32 Zokolola Zoculuka ! Pamene Mulungu anali kulenga dziko lapansi ndi zinthu za m’dziko , Mwana wake wobadwa yekha anali pambali pake monga “ mmisili waluso . ” ( Miy . 8 : 22 , 30 , 31 ; Akol . Ciphunzitso ca Akatolika cimati kuloŵana m’malo kwa atumwi kwapitilizabe kucokela m’nthawi ya mtumwi Petulo kudzafika m’nthawi ya apapa . Tikakumbukila nthawi yokondweletsa imeneyo , naise timalimbikitsidwa kukamba kuti , “ Zikomo kwambili Yehova cifukwa conipatsa mwayi wopezekapo . ” Anasimba motelo Alona . Ana anga anayi , James , Jerry , Nicholas , ndi Steven , akutumikila Yehova mokhulupilika pamodzi na mabanja awo . Koma bwanji ngati simukwanitsa kucita ulaliki mmene mufunila cifukwa ca kudwala kapena ukalamba ? 16 , 17 . ( a ) Kodi anthu osakhala Ayuda anapindula motani cifukwa ca Ayuda okhala m’madela ena ? Kuwonjezela pamenepo Yehova anayamba kum’patsa Yobu zonse zimene anali nazo , kuwilikiza kaŵili . ” ( Yak . 5 : 7 , 8 ) Ngakhale kuti mbeu zimene tinabyala sizikubala zipatso , ndipo tacita zonse zotheka kuthandiza wophunzila wathu , koma sakupita patsogolo , sizitanthauza kuti tilibe cikhulupililo . Ni mapindu anji amene timapeza tikakhala oceleza ? Komabe , Akristu odzozedwa anali kuyembekezela mwacidwi kutha kwa “ Nthawi za Akunja , ” kapena kuti “ nthawi zoikika za amitundu , ” m’caka ca 1914 . Kunena zoona palibe amene anapezapo mankhwala a moyo . Komabe , banja lililonse lili na ufulu wodzisankhila lokha njila imene ingathandize ana awo kukhala olimba kuuzimu . Baibulo limafotokoza zimene zidzayamba kucitika padziko lapansi Mulungu asanaononge anthu oipa . Kwa zaka zambili ndinali kupemphela kuti umoyo wa banja lathu ukhale wabwino . Sitingathe kukakamiza kuti mbeuzo zikule kapena kuzifulumizitsa . Yehova akanakwanitsa kugwila yekha nchitoyi . Kwa Zaka 58 zimene tinatumikila pamodzi ndi mkazi wanga , tinaona ciŵelengelo ca anthu a Yehova ku Puerto Rico cikukwela kucoka pa 650 kufika pa 26,000 . TSIKU lina m’maŵa ku Brookings , m’dela la South Dakota , ku U.S.A , kunazizila , ndipo ine n’nadziŵilatu kuti posacedwa kudzazizila kwambili . Mogwilizana na lonjezo lake , wanipatsa mphamvu , kunilimbikitsa , ndi kunigwila na ‘ dzanja lake lamanja lacilungamo . ’ — Yes . Cifukwa ca cifundo , iye “ anayamba kuwaphunzitsa zinthu zambili . ” Panthawiyo , Amidiyani amene anali kukhala moyandikana ndi Aisiraeli anali pa udani woopsa ndi Aisiraeliwo . ( 2 Akor . 13 : 5 ) Pali zocita zathu zina zimene nthawi ndi nthawi zimafuna kuzifufuza , kuti tikhale otsimikiza mtima kuti kulambila kwathu n’kopanda cinyengo . Kwa nthawi , Davide anapitiliza kugwila nchito yake yoŵeta nkhosa . ( Yohane 5 : 28 , 29 ) Malonjezo amenewa ndi osangalatsa kwambili . Kuwonjezela pamenepo , cikwati cimeneci cidzacitikila kumwamba . Kodi Nowa anacita ciani na zimene akanakwanitsa kucita ? M’nkhani yotsatila , tidzakambilana makhalidwe ena amene munthu amakhala nawo ngati ali na cikondi cadyela . Tidzaonanso mmene makhalidwewo alili osiyana ndi makhalidwe a atumiki a Yehova . Paulo na Baranaba anaika miyoyo yawo paciswe mwa kubwelelanso kumene anamenyedwa . Kungolalikila mwacizoloŵezi anthu samvetsela . Ana ambili osamalila makolo amakhala ndi cisoni , nkhaŵa , ndipo angakwiye ndi kukhumudwa . ( Aheb . 10 : 32 - 34 ) Paulo anayelekezela mayeselo amene Akhiristu amalimbana nawo ndi maseŵela a mpikisano amene Agiriki anali kucita . Cikhulupililo ca Mkhiristu cimazikidwa pa mfundo yakuti Yehova ni “ Mulungu wokhulupilika , ” amene amakwanilitsa zimene walonjeza . — Deut . Mwacitsanzo , Yesu anakamba za “ cizindikilo ca mneneli Yona . ” Zimenezi ziyenela kuti zinawalimbikitsa ngako Ayuda amene anali kumanga kacisi m’nthawi ya Zekariya . Mwacitsanzo , pamene inu muona kuti Mkristu wina ndi wolakwa kwambili , Mulungu angaone zinthu mosiyana . Kuti mudziŵe mtundu wa kosi imene mungacite , funsani woyang’anila dela ndi apainiya m’dela lanu . Anamuika m’ndende na kum’manga maunyolo . — Genesis 39 : 1 - 20 ; Salimo 105 : 17 , 18 . Azibweletsanso mwana wa nkhunda kapena njiŵa kuti ikhale nsembe yamacimo . ” ( Mac . 8 : 14 ; 15 : 2 ) Akhristu a ku Yudeya anali kulalikila za Khristu kwa anthu amene anali kukhulupilila kale mwa Mulungu mmodzi . ( Lev . 19 : 2 , 11 ) Komabe , munthu angamapewe mabodza apoyela , koma n’kumagwila ena m’maso , kumawapita pansi . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Valani cifundo cacikulu , kukoma mtima , kudzicepetsa , kufatsa , ndi kuleza mtima . ” — Akolose 3 : 12 . M’kanthawi kocepa cabe , Yobu anatayikilidwa anchito ake , katundu , ndi ana ake 10 . Danieli sanafune kusintha maganizo ake pankhani yolambila Mulungu woona . Kuti mumvetse bwino mmene ulosiwu unakwanilitsidwila mu 1914 , onani buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni masamba 215 mpaka 218 . Kuyambila m’ma 1990 , takhala tikusangalala kwambili na ufulu wolalikila uthenga wabwino na kusonkhana pamodzi mwaunyinji . Kodi simuvomeleza kuti makhalidwe amenewa akuwonjezeleka masiku ano ? Nkhani yapoyela imene inali italengezedwa , ya mutu wakuti “ Kugwetsedwa kwa Ulamulilo wa Satana , ” inakoka “ anthu acidwi pafupi - fupi 300 . ” Paulo analangiza Timoteyo kuti : “ Ukhale ndi cizoloŵezi cocita zinthu zokuthandiza kuti ukhalebe wodzipeleka kwa Mulungu . ” ( 1 Tim . Mulungu sanapange anthu kuti azifa , koma kuti akhale na moyo kwamuyaya . Tinaphunzila mocitila phunzilo laumwini lopindulitsa , na mofufuzila mfundo zina zofunika . Nanga bwanji za amene ali ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi , amene anacilikiza odzozedwa pa nchito yolalikila ? Iwo adzakhala ataweluzidwa kuti ndi nkhosa , ndipo adzapatsidwa mphoto yokhala ndi moyo padziko lapansi mu ulamulilo wa Ufumu wa Mulungu . — Mat . Komabe muyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ndidzacita ciani ndi moyo wanga tsopano ndikaliko ndi mphamvu ? ’ Abwana anandilolanso , ndipo codabwitsa n’cakuti malipilo anga anali amodzimodzi . Koma afunanso kuti timasuke ku zizoloŵezi zimene zimaipitsa maganizo athu . Akhristu amene anavala umunthu watsopano amalemekeza Akhristu anzawo ndi anthu ena mosasamala kanthu kuti ni a mtundu wanji , olemela kapena osauka . Atate wathu wacikondi amafuna kuti tizitsatila njila yacilungamo , koma samatikakamiza kucita zimenezi . Anthu ena ouma mtima anali kulanda munthu covala ngati ali naye nkhongole , n’kumusiya alibe ciliconse cakuti angafunde pogona . Zoona Yehova ni wokhulupilika , ndipo amakwanilitsa malonjezo ake . Nthawi zina , angacite zimenezo m’njila imene ingatidabwitse kapena kuikaikila . Tsiku lotsatila , maganizo atakhazikika tinakambilana bwinobwino ndi mwana wathu , ndipo tinam’fika pa mtima . nchito yabwino ? 7 : 28 ) N’zomvetsa cisoni kuti anthu ambili m’dzikoli amaona cikwati mopepuka . Ndithudi , tifunika kuonetsa khalidwe la kupanda tsankho mocokela pansi pa mtima osati mwaciphamaso . ( Yuda 20 , 21 ) Nanga tingaonetse bwanji kuti tikuyembekezela mwacidwi lonjezo la Mulungu la paladaiso ? ( Mlal . 3 : 7 ) Mlongo wina wamasiye , dzina lake Dalene anati : “ Anthu amene afedwa amafuna kufotokoza maganizo awo ndi mmene amvelela . ( Mateyu 6 : 25 , 27 ) Koma , kodi tingacite ciani kuti tileke kuda nkhawa ? Mbonizo pogwilitsila nchito Baibulo , zinandionetsa cifukwa cake anthu sangakwanitse kuthetselatu kupanda cilungamo ndi nkhanza . Tingatengele bwanji cikhulupililo ndi kumvela kwa Yobu ? Nkhani iyi itithandiza kudziŵa zimene tingacite kuti tipindule ndi lemba la caka cino . Zimenezi zimatisiyanitsa ndi anthu ambili m’dzikoli . Mofanana ndi Kevin , tifunika kupitilizabe kusintha umunthu wathu . Lelolino , anthu ambili akali ocititsidwa khungu na mulungu wa nthawi ino ndipo ni akapolo a cuma , cipembedzo conama , na cikhalidwe cawo . ( 2 Akor . Yesu pokhala munthu wangwilo , anali ndi moyo wamuyaya monga wa Adamu asanacimwe . Analinso ndi ana ambilimbili a kuuzimu . 14 - 16 . Kodi Yehova anasintha zocitika za padziko n’colinga cakuti Akristu akwanitse kulalikila m’nthawi ya atumwi ? Baibulo silinena ciliconse pankhaniyi . Njila imene Sara anaona kuti ingathandize ikanam’bweletsela mavuto . Tikamapemphela timayandikila Yehova . Conco , kungakhale kupanda nzelu kumasinthasintha machanelo kuti tione mapulogalamu amene alipo . Colinga cinali cakuti wina akapita ku sukulu , wina azitsala pa nyumba kusamalila ana na kukonza cakudya cam’madzulo , kuti atate pobwela ku nchito azipeza zonse zili m’malo . Cifukwa ca zimenezi , tinayamba kuphunzila Baibulo pamodzi ndi mnyamatayo . Ndipotu tsitsi lenilenilo la m’mutu mwanu amaliŵelenga . Tiphunzilapo ciani pa zimene zinacitikila Mose ? Sitiyenela kuganiza kuti kukamba moona mtima n’kupanda ulemu . Mnyamatayo atamva zimene amai ake anakamba , anadziŵa kuti anali kukhulupililabe kuti angathe kusintha . CISONI NA KUVUTIKA MAGANIZO CUMA CIKASILA . Niuzeni ! ” WASAYANSI , DR . Koma kaya tidzakumana ndi zotani , tili ndi cidalilo cakuti Yehova sadzatisiya . ( Deut . Ngati wanchito wamba anali kulandila dinari imodzi patsiku , ndiye kuti akanafunika kugwila nchito zaka 20 kuti alandile talente imodzi . Munandiphunzitsa zinthu zambili zabwino . Dziŵani kuti Yehova adzatipulumutsa ku dongosolo la zinthu loipali ndi kutipatsa moyo wosatha . — 1 Pet . Timaona kuti Yehova anamva pemphelo lathu . Nanga inu zinthu zili bwanji pamaso pa Mulungu ? Satana Mdyelekezi , amene ni “ wolamulila wa dziko , ” ndiye amacititsa mavuto ambili . — Yohane 14 : 30 . Stephanie anayankha kuti : “ Kukamba zoona , kulalikila m’gawo limene anthu amafunitsitsa kuphunzila coonadi , ndipo ni okonzeka kuphunzila Baibulo tsiku lililonse , n’kosangalatsa kwambili . komanso anthu amene amva zimenezi amanenanso kuti “ Bwela . ” Mabuku ofotokoza Baibo amenewo ananithandiza ngako kuti nisinthe na kukhala Mboni ya Yehova . Loraini ndi Jenny anali kutumikila limodzi pa nthambi ya ku Fiji . Tsiku lina , mokhumudwa ninawauza kuti sitidzaphunzila apite kucipinda cawo akagone . Kodi khalidwe la Afarisi linali losiyana bwanji na cifundo ca Mulungu ? Kuwonjezela pa kufotokoza za malo ake okwezeka , Malemba amaonetsa kuti Yesu , mofanana ndi Yehova , amatikonda kwambili . Ni umboni uti wa cikhulupililo umene tiona masiku ano ? Nanga n’ndani ayenela kulemekezedwa cifukwa ca izi ? Mmene mumaonela ena : Kodi mu mpingo mwanu muli wina amene zocita zake sizikukondweletsani ? ( b ) Tiyenela kuiona bwanji nkhani ya kumwa zoledzeletsa tisanacite zinthu za kuuzimu ? ( a ) Kodi colinga ca Satana n’ciani ? N’tapezeka pa msonkhano wa Mboni za Yehova , mkazi wanga ananiuza kuti nisankhepo pali kuleka kuphunzila Baibulo kapena kuthetsa cikwati . Cimodzi cimene mungacite ni kulabadila malangizo a pa Afilipi 2 : 3 , pamene pamatilimbikitsa kukhala ‘ odzicepetsa , ndi kuona ena kukhala otiposa . ’ N’kutheka kuti m’maso mwa Davide , Solomo anam’cepela kuti angayang’anile nchito yofunika kwambili imeneyo . N’ciani cionetsa kuti mpingo wacikhiristu woyambilila unali wadongosolo ? ( Mateyu 4 : 4 ) Palembali Yesu anali kunena za nthawi pamene Aisiraeli anali kudalila Mulungu kuti awapatse zofuna zao , atangocoka mu Iguputo . “ Kuleza mtima , kukoma mtima , ubwino . ” Kodi mmene Yehova anatilengela zimaonetsa bwanji kuti amatikondadi ? ( Onani nkhani yapita . ) 4 : 15 . Akhristu oyambilila anakhala na mbili yabwino yakuti anali kukondana . Cifukwa cakuti n’coleza mtima , n’cokoma mtima , komanso cimakhululuka , cikondi cimeneci “ cimagwilizanitsa anthu mwamphamvu kwambili kuposa cinthu cina ciliconse . ” Mwacitsanzo , ngakhale kuti mtumwi Paulo anali wocita bwino m’zambili , anali na zofooka zina zimene zinali kumulepheletsa kucita zonse zimene anali kufuna . ( a ) N’zocitika ziti zimene zingacititse makolo kubwelela ku mpingo wa cinenelo cimene ana awo amamvetsetsa ? 51 : 17 ) Komabe , ena ocepa sanalape . Nkhosa ya pasika imene Aisiraeli anali kupha inali kuimila cinacake . — Num . Ngati timayesetsa kusintha kuti tikondweletse Yehova , timaonetsa kuti timam’kondadi NYIMBO : 38 , 69 Kuŵelenga Baibo tsiku lililonse ( 2 Akor . 10 : 7 - 12 ; 12 : 11 - 13 ) Kodi tiyenela kucita ciani ngati ena ayamba kutsutsa otsogolela mumpingo ? “ Koma dziŵa kuti , masiku otsiliza adzakhala nthawi yapadela komanso yovuta . Masiku ano , tamalimvetsa bwino fanizo la nkhosa ndi mbuzi . Nikumbukila kuti nthawi ina n’nali kufufuza m’magazini a Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani * nkhani za anthu amene anakwanitsa kusintha umoyo wawo monga mmene ine n’nafuna kucitila . Ni mauthenga osoceletsa . Poyamba zinanivuta kuti nim’khululukile . Ise sitifuna kukhala na makhalidwe monga amenewa . M’malomwake , timafuna kukhala na cikondi , cimene “ sicisamala zofuna zake zokha . ” — 1 Akor . Iye anati : “ Osakamba ndi ine . Ngakhale n’conco , kukali gawo lalikulu losalalikidwa . Mwacitsanzo , kupyolela mwa Yesaya , Yehova anakamba kuti : “ Tsatilani cilungamo ndipo citani zolungama . . . Tiyenela kutengela citsanzo ca Yehova mwa kupewa kukhala “ wolungama mopitilila muyezo ” mpaka kukana kulandila ocimwa amene abwelela mumpingo . Mayi wina wacisurofoinike anafikila Yesu Kristu ku dela la Sidoni mwamsanga pambuyo pa Pasika wa mu 32 C.E . 1 Samueli caputa 25 Iye sanaike malile a nthawi imene tiyenela kukamba naye . Kumbukilani kuti Yehosafati anali mfumu yabwino ndithu . 10 : 18 ) Ni mwayi waukulu kuimila Yesu m’njila imeneyi . Rakele Anali Kulilila Ana Ake ( Yer . ( Ŵelengani Mika 6 : 8 . ) 3 : 15 ) Kukhala ndi “ cikondi ceniceni ” kungathandize okwatilana “ kukhala patsogolo ” pankhani yosamalilana ndi kupatsana ulemu . — Aroma 12 : 10 . ( Mac . 3 : 19 ) Kukamba zoona , ngati munthu wadzipeleka kwa Mulungu pamene akucitanso macimo aakulu amene angamulepheletse kukaloŵa mu Ufumu , ndiye kuti kudzipeleka kwake n’kosayenela . ( 1 Akor . Komabe , ife timadziŵa kuti Yehova amakondwela ngati timuyamikila pa zinthu zimene watipatsa . M’kupita kwa nthawi , anaona kuti kukonda zosangulutsa kunam’bweletsela mavuto ambili . Iwo anati , “ Usakayese kugwilizana nao anthu amenewo ! ” Anthu adzapitiliza kukumbukila ndi kutamanda mfumuyo ku mibadwo yonse yobwela mtsogolo . Njila imodzi imene tingacitile zimenezi ndi mwa kugwilitsila nchito nthawi yathu , mphamvu zathu , ndi cuma cathu polambila Yehova ndi pothandiza ena kudziŵa za iye . Conco , pamene Yehova anauza Abulahamu kuti apeleke mwana wake nsembe , Abulahamu anadziŵa kuti nthawi zonse Yehova anali kumucitila zinthu moleza mtima , mwacifundo , mokhulupilika ndiponso anali kumuteteza . [ Zinenelo 120 ] 3 : 16 - 18 , 20 , 28 ; 6 : 13 , 16 , 21 - 23 . Mwacitsanzo , iye atagonjetsa adani a Mulungu kunkhondo , anatenga milungu yawo ndi kuyamba kukailambila . — 2 Mbiri 25 : 11 - 16 . Cimene ndikungofuna n’cakuti ndimalize kuthamanga mpikisano umenewu , komanso kuti ndimalize utumiki umene ndinalandila kwa Ambuye Yesu basi . M’bale Jason , amene tamuchula kuciyambi , anati : “ Pa nthawi yonse imene nakhala mkulu , naphunzila zambili ndipo sinidzikayikilanso posamalila udindo wanga . Iye ni wofunitsitsa kutithandiza na kutilimbikitsa kuti tilimbane na mavuto . Acibale angasonyeze kuti amakonda mpingo ndi munthu wolakwayo mwa kulemekeza cigamulo ca kucotsa munthuyo . Ganizilani mmene timapindulila cifukwa ca kuŵelenga Baibo , kuphunzila zofalitsa za “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu , ” kutamba TV yathu yochedwa JW Broadcasting , ndi kuyanjana ndi Akhristu anzathu . Timapindulanso kwambili na webusaiti yathu ya jw.org , komanso malangizo amene akulu amatipatsa . ( Mat . Kodi moyo uli ndi phindu lililonse ? “ Kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” wakhala akufalitsa nkhani zosiyanasiyana . ( Mat . Akristu sangafunike kulekelatu kumwa moŵa , kuvina kapena kulekelatu kucita zinthu zina zimene sizolakwika . Marthe , * mlongo amene anavutika maganizo kwa nthawi itali , analemba kuti : “ Tsiku lina pamene n’napemphela kuti nipeze cilimbikitso , n’nakumana na mlongo wina wacikulile amene ananionetsa cikondi na cifundo . Ngakhale n’conco , iye sanagonje , koma anaonetsa kulimba mtima mwa kum’thawa mkaziyo . — Gen . Ndiye cifukwa cake tifunika kukonzekela kuti tidzapewe kutenga mbali m’ndale za dziko losagwilizanali . Ngakhale kuti zinali zovuta kupeza malo abwino okhala ndi nchito yamaziko , iye anali kuphunzitsa Cijapanizi ndi kugwila nchito yoyeletsa kuti azizithandizila pocita upainiya . Munthu amene wakupatsani magazini ino adzakuuzani nthawi ndi malo kumene kudzacitikila Cikumbutso m’dela lanu , kapena mungafufuze pa Webusaiti yathu ya jw.org . ( Mat . 6 : 33 ) Malemba amatikumbutsanso udindo na mwayi umene tili nawo wolalikila kunyumba ndi nyumba , mwamwayi , ndi ulaliki wapoyela . ( Mat . 28 : 19 , 20 ; Mac . Coyamba , muziika patsogolo zinthu zofunika kwambili . Kum’mwela kwa Africa ndi ku Central America , ndi kumene kunaphedwa anthu ambili ( anthu 30 pa anthu 100 , 000 aliwonse ku Southern Africa , ndi anthu 26 pa anthu 100 , 000 ku Central America . ) Nkhani zotsatizana za m’magazini ino , zafotokoza mmene Baibulo inapulumukila . Pa nyumba pathu pali mtendele . ( Luka 19 : 11 - 13 , 15 ) Yesu anafotokozelanso atsogoleli aciroma kuti iye sali mbali ya dziko . Kodi mungatsatile bwanji malangizo a Yesu kuti mucepetse nkhawa zozizilitsa m’nkhongono ? Zoonadi , Yehova sadzaleka kukonda atumiki ake . Poona kuti cosankha cawo pa nkhaniyi cidzakhudza umoyo wawo wonse , acicepele ambili amakopeka na mfundo zimenezi . Mwacitsanzo , wacicepele wobatizika wosinkhukilako angayambe kukopeka na zinthu za m’dzikoli , kapena angayambe kukayikila ngati kutsatila mfundo za m’Baibo n’cinthudi coyenela . Pitilizani kuŵelenga kuti mudziŵe . ▪ Kodi N’zotheka Kukhala m’Cikondi Ceniceni ? mmene Yehova amatithandizila kukwanilitsa utumiki wathu ? Popeza kuti Nowa , Danieli , na Yobu anafuna - funa Yehova na mtima wawo wonse , iye analola kuti iwo am’peze . Pangano la Abulahamu linakwanilitsidwa koyamba kwa mbadwa zake , pamene zinaloŵa m’Dziko Lolonjezedwa . Komabe , Malemba amaonetsa kuti mbali ina ya pangano limeneli ili ndi kukwanilitsidwa kwa kuuzimu . Muziyang’ana kwambili pa makhalidwe ake abwino , ndipo muzimuyamikila . Nthawi yovuta ino idzasila manje - manje . “ MULI BWANJI ? ” Kuti mucimvesetse cimwemwe , ganizilani za thanzi labwino . Mwacitsanzo , nthawi zambili timapita ku Khoti Loona za Ufulu wa Anthu ku Ulaya . Iwo anacita zinthu mopitilila malile posalemekeza udindo wa Akhristu anzawo wodzipangila zosankha . Nanga bwanji za nthawi pamene ciweluzo cidzacitika ? Nayenso mtumwi Paulo anapeleka citsanzo cabwino kwambili mwa kudzipeleka na kugwilitsila nchito nthawi yake pothandiza ena . Muziyanjana ndi abale ndi alongo anu . Pamene mupita patsogolo kuti mukwanilitse colinga canu , mudzakondwela kutumikila Yehova . Zimenezi zinandithandiza kwambili paumoyo wanga . Patsikulo , iye anauka monga mkaidi wonyozeka koma anagona monga wolamulila waciŵili kwa Farao . Ngakhale kuti akanakhala ndi maganizo amenewo , iye anacilikizabe kulambila koona mmene akanathela . Cilamulo ca Mose cinati : “ Munthu akalonjeza kwa Yehova , kapena akacita lumbilo . . . , asalephele kukwanilitsa mau ake . 68 : 11 . Koma Yosefe anali kudziŵa kuti mtembo wa Yesu sungaikiwe m’manda mwaulemu ngati sipapezeka munthu wokapempha Pilato kuti apeleke cilolezo cocotsa mtembowo . Kodi ndiyenela kufufuza zina zowonjezeleka pankhaniyi ndi kukambitsilana ndi anthu amene anaphunzila za udokotala kuti andithandize ? ’ — Deuteronomo 17 : 6 . Onani malonjezo a m’Baibo awa . Kodi ubatizo wathu umaonetsa ciani ? Carson analemba kuti , liu lacigiliki lakuti “ kacisi ” lopezeka m’buku la Mateyu ndi Luka , lingatanthauze malo onse a pa kacisi osati cabe malo opatulika a pakacisi , amene Alevi okha anali kuloledwa kuloŵamo . Ndipo cikondi cathu pa Mulungu ‘ cimakhala cokwanila ’ pamene timvela lamulo lakuti tizikonda ena , maka - maka Akhiristu anzathu . — 1 Yoh . 4 : 12 , 20 . “ Ine ndasautsika ndipo ndasauka . Katherine anati : “ Mau a a Doris anali yankho la pempho langa . Kucita zimenezo , kumathandiza kuongolela maganizo olakwika a ana ao ndi kuwathandiza kuti akule bwino . ( Mateyu 5 : 3 ) Kunenadi zoona , anthu mwacibadwa amafuna kudziŵa Mulungu . Onani buku lakuti “ Kuchitila Umboni ” Mokwanila za Ufumu wa Mulungu , mutu 16 , ndime 5 - 6 . Ngakhale kuti Ayudawo anali kukhala m’madela osiyanasiyana , io anapitilizabe ndi cipembedzo cao . — Mat . Izi zinacititsa kuti Yobu ayambe kuganiza kuti Mulungu ndiye anali kucititsa mavuto ake . 25 : 20 - 23 . YEHOVA MULUNGU analenga anthu ndi ufulu wodzisankhila zocita . Nanga abale amene akulila ku Micronesia , apindula bwanji ndi thandizo limene amalandila ? Munthu angayamikile maningi mphatso imene walandila olo kuti ni yochipa , malinga ngati yamuthandiza pa cosoŵa cake . 4 : 8 ) Zimenezi n’zolimbikitsa kwambili . 3 : 1 - 5 . Nkhani zimenezi zimapezeka nthawi ndi nthawi mu Nsanja ya Olonda yogaŵila . Kwa mwana wosinkhulilapo , mungamufotokozele kuti lesipi ya apozi — kapena ya mtengo wake weniweniwo , inalembedwa mu DNA yake , kapena kuti m’majini ake . 5 : 20 . N’zoonekelatu kuti nkhani yokhudza paradaiso wotaika padziko lapansi yakhala yodziŵika kwambili m’mbili yonse ya anthu . Cifukwa cakuti m’baleyo anali kufotokoza mwaulemu , zinathandiza kuti kazembeyo aziiona moyenela nchito yathu na kuleka kuizonda . 5 : 43 - 48 ) Lamulo lakuti tizikonda mnansi wathu ni laciŵili pa lamulo lakuti tizikonda Yehova . Yesu sanacite manyazi kuonetsa mmene anali kumvelela . 6 : 13 ) Khama lake lophunzila cineneloco linacititsa kuti abale am’konde kwambili . Tiyelekezele kuti Mkhristu mnzanu anakukhumudwitsani , ndipo mukulephela kuiŵalako zimene anakucitilani . 24 : 3 ) Komabe , pasanapite nthawi , panacitika zinthu zina zimene zinayesa kukhulupilika kwawo kwa Yehova . 11 , 12 . ( a ) M’nthawi ya atumwi , n’ciani cionetsa kuti Yehova anakana mtundu waciyuda ndi kuyamba kuyanja gulu lina ? Ndife osangalala cifukwa cakuti tikudziŵa bwino zimene zikucitika . Paulo anagwilitsila nchito ufulu wake monga nzika ya Roma pa zocitika zingapo . N’cifukwa ciani zili conco ? 7 , 8 . ( a ) Kodi Akristu masiku ano ali ndi mwai wogwila nchito yotani ? Yosimbidwa ndi Trophim R . Pamene tikambilana mafunso amenewa , tidzaonanso zimene tingaphunzilepo . Zimenezi n’zofanana ndi mkazi amene wakwatiwa ndi mfumu . Iye akakwatiwa , amalamulila ndi mfumuyo . Ifenso tiyenela kumvela uphungu umenewu . — 3 Yoh . 11 . Ndipo timafunika kukwanilitsa malonjezo athu kuti Mulungu apitilize kutikonda . Anthu ena amaganiza kuti kugwedeza thupi kapena ziwalo zina za thupi pofuna kukopa ena , kucita magesica okopa , ndi kuyang’ana kokopa kulibe vuto cifukwa anthu sagwilana . 5 : 43 , 44 . 32 : 4 ; Sal . 145 : 17 ; Yak . Mulungu analonjeza mwana wa Abulahamu , Isaki ndi mdzukulu wake , Yakobo kuti adzawadalitsa ndi kuti m’banja lao mudzatuluka mafumu . ( Gen . Yesu anali kudziŵa kuti ngati ophunzila ake acita khama potumikila Yehova ndi polalikila uthenga wabwino , adzakhala osangalala kwambili . ▪ Khalani Wolimba Mtima ndi Wozindikila Monga Yesu cithandizo ca mankhwala ? Conco , n’tatsiliza zaka ziŵili , mu 1956 n’naileka . Zomela ndi nyama padziko lapansi zimadalilana . Atangomuona cabe , anazindikila kuti anali kulila . Popeza ndinali kudziŵa zaulimi , anandipempha kuti ndizigwila nchito pa famu ya pa Beteli imene inali kugwila nchito panthawiyo . 3 , 4 . Kwa zaka 20 zapitazo , io akhala akuyenda m’maiko ambili a mu Africa kuthandiza pa nchito yomanga Nyumba za Ufumu . Mipingo yambili inacita zimenezi , ndipo ofesi ya nthambi inalandila malipoti ambili abwino ponena za makonzedwe amenewa , ngakhale kucokela kwa anthu amene si Mboni . Kodi tiphunzilapo ciani pa cocitika cimeneci ? Mukatelo , mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu . ” ( Afil . Patangopita nthawi yocepa , Yehova anaweluza Ahabu . Colinga ca Satana ndi kuononga ubale wathu ndi Yehova . 8 , 9 . ( a ) Ni makhalidwe ati amene tiyenela kukhala nawo kuti tikalandile mphoto ? ( Aroma 1 : 16 ) Muziyesetsa kukambilana ndi aphunzitsi ao za nkhani zimenezi ngati m’pofunika kutelo . Ali ku nkhondoko n’kutheka kuti anapeza cofalitsa ca Ophunzila Baibulo na kuciŵelenga . Gulu loyamba ndi Akristu odzozedwa amene anali ndi moyo mu 1914 , ndipo anazindikila kuti Yesu anayamba kulamulila m’cakaco . Inde , anali na mwayi wokhala na umoyo wacimwemwe ndi wokhutilitsa . Panthawiyo , Yesu anali atangoukitsidwa kumene . Si tuakacisi tonse tumene tungakhale malo olambililapo acipembedzo . Fotokozani citsanzo ca mtumiki wa Mulungu wamakono pa kaonedwe kabwino ka zinthu . Tipeza yankho pa zimene Paulo anauza akulu a mpingo wa ku Efeso . Mwacidule , tifunika kucita zonse ziŵili , kudalila Yehova ndi kucita zabwino , kapena kuti kucitapo kanthu mokhulupilika . M’Baibo simudzapezamo mau akuti “ mzimu wosafa ” M’Baibulo muli uphungu wothandiza a m’cikwati kukhala oganizilana pa nkhani ya kucipinda . Ngati titengela cikhulupililo ca Debora , mwa kukhala kumbali ya Yehova molimba mtima ndi kulimbikitsa anthu ena , Yehova adzatiteteza ndipo tidzakhala ndi mtendele wosatha . Tiyamikila kwambili kuti Yesu wasunga lonjezo lake lakuti adzasamalila zosoŵa zathu za kuuzimu . ( 1 Akor . 5 : 11 - 13 ) Ngakhale kuti cimaŵaŵa mumtima , tifunika kupewa kukambitsana kosafunikila ndi wa m’banja wocotsedwa , kaya m’pa foni , pa meseji , m’kalata , kapena pa intaneti . Iwo anandikakamiza kuti ndisiye kuphunzila Baibulo ndi kusonkhana . Kucita zimenezo kungakhale kovuta . Cocitika ca Elisa amene analowa m’malo Eliya cimaonetsanso mmene abale masiku ano angasonyezele ulemu kwa akulu amene atumikila kwa zaka zambili . PANAYIOTA anakulila pacilumba cina ca ku Mediterranean . Iwonso angapindule na malangizo a pa Aroma caputa 8 opita kwa anthu olungama . N’cimodzi - modzi na ise . ▪ Kodi Muli pa Ubwenzi Wolimba ndi Yehova ? Mateyu anachula maina a makolo a Yosefe ndi kuonetsa kuti Yesu , mwana wa Yosefe , anali woyenelela mwalamulo kuloŵa ufumu wa Davide . Anthu adzakhala ndi moyo wosatha padziko lapansi cifukwa cokhulupilila nsembe ya dipo ya Yesu . ( Yoh . Kucita zimenezi kudzakuthandizani kupewa kucita zinthu mopupuluma . ( Miy . Kodi Ophunzila Baibo anatenga kaimidwe kotani molimba mtima kulinga kwa Babulo Wamkulu ? Ngakhale kuti sindinali kutsutsa zakuti Mulungu aliko , panali nkhani zina zimene zinali kundizunguza mutu . Ngati ndinu wacinyamata wazaka zosakwana 20 kapena kuposelapo pang’ono , kodi cinthu cofunika kwambili kwa inu n’ciani ? Amafufuza mfundo za m’Baibulo zimene zingamuthandize kusiyanitsa cabwino ndi coipa . Iye amacita zimene angathe kuti alimbikitse mgwilizano mumpingo Iye ndi banja lake anatangwanika ndi kucita cifunilo ca Mulungu kuphatikizapo kumanga cingalawa . Pasanapite nthawi yaitali , anthu anayambanso kupandukila ulamulilo wabwino wa Yehova . 1 : 42 . Nanga mwatsimikiza mtima kucita ciani ? Kodi mungadziŵe bwanji kuti n’zoona ? ( Sal . 24 : 3 , 4 ; 51 : 6 ; Afil . Patapita masiku ocepa , mwini malowo anauza banjalo kuti lisacoke pamalopo . Mosasamala kanthu za kumene tidzatumikila kapena zimene tidzacita , ndife otsimikiza kuti tidzakhala oyamikila , okhutila , ndiponso osangalala kwambili . — Neh . Ndithudi , Mulungu sakondwela ndi kucitila akazi nkhanza . Ngakhale kuti timadana ndi khalidwe limeneli , mosazindikila tingayambe kuwaona mosayenela anthu ofooka amene amafunika thandizo . Ndipo tingacite zimenezi ngakhale kwa abale athu mu mpingo . ( 2 Timoteyo 3 : 15 ) Ndiyeno mukuganiza kuti : ‘ Kodi mau amenewa akupezeka pati ? ’ ( Mat . 6 : 24 ) Popeza ndise opanda ungwilo , tonse tifunika kupitiliza kulimbana ndi “ zilakolako za thupi lathu , ” kuphatikizapo mzimu wokonda cuma . — Aef . Koma angalandile mokondwela mphatsoyo cifukwa ionetsa kuti mwanayo amam’konda . Ndipo kapepala kakuti , Kodi Cofunika N’ciani Kuti Banja Likhale Lamtendele ? , kamatsogolela m’phunzilo 9 . Koma buku la Luka limafotokoza kwambili za Mariya . ( Sal . 23 : 1 - 3 ) Iye ndiye “ pothawila pathu ndi mphamvu yathu , ” makamaka panthawi ya masautso . Abulahamu anadziŵa kuti ngati wamvela Yehova , Iye adzamudalitsa limodzi ndi mwana wake . 9 : 11 ) Mukaganizila zimene zinacitikazo , n’kutheka kuti mumadzifunsa kuti , ‘ N’cifukwa ciani Yehova analola zimenezi kunicitikila ? ’ Ndinali kufunabe kumvetsetsa Baibulo ndipo ndinapempha Mulungu kuti andithandize . Nkhondo ya Aramagedo ikadzayamba , sitidzafunika kumenya nkhondo yolimbana ndi adani athu . Zinthu zambili zimene dzikoli limafalitsa ndi kuulutsa zingaononge Akristu mwakuuzimu . NYIMBO : 56 , 138 Kodi zocitika zimene zinalembedwa pa Salimo 45 zimakhudza bwanji Akristu onse oona masiku ano ? M’Baibo , kudzicepetsa kumatanthauzanso kusadziika pamene suli , komanso kudziŵa bwino zimene sungakwanitse . Zimenezi zinacititsa cidwi m’bale ameneyu . Mpingo wathu unafika pogula basi kuti tizikwanitsa kukalalikila ku matauni ndi ku midzi ina yoyandikana ndi tauni yathu kumapeto kwa wiki iliyonse . 4 : 7 , 8 ) Kodi tiyenela kutani ndi malangizo amene amatipatsa ? ANTHU ENA AMAKHULUPILILA kuti nthawi zonse tifunika kugwada , kuŵelama , kapena kuika manja pamodzi popemphela . Brook anati : “ Ngakhale kuti nthawi zina apainiyafe timakumana ndi mavuto , timakhalabe okhutila ndi umoyo wathu . Wallis anati : “ Kuthela maola 5 mu ulaliki kwa masiku angapo mu wiki kunali kokondweletsa kwambili . Baibulo limaonetselatu kuti Mulungu sanatilenge m’njila yakuti tizidzisankhila cabwino ndi coipa . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mafanizo ena atatu ndi kuona zimene tikuphunzilapo . Iye anaona kuti afunika kusintha khalidwe lake . Conco , anapepesa m’bale amene anali kukangana naye , ndipo anayesetsa kulamulila mkwiyo wake . N’cifukwa ciani io anali kupita ku malo amenewa ? 28 : 19 , 20 ) Pokambilana na atumwi komanso ena mwa ophunzila ake , iye anati : “ Ngati munthu akufuna kunditsatila , adzikane yekha ndi kunyamula mtengo wake wozunzikilapo ndipo anditsatile mosalekeza . ” — Mat . UFUMU WA KHRISTU — BOMA LA PADZIKO LONSE LACILUNGAMO : ‘ Yesu Khristu anapatsidwa ulamulilo , ulemelelo , ndi ufumu kuti anthu a mitundu yosiyana - siyana , olankhula zinenelo zosiyana - siyana azimutumikila . ( b ) Ni makhalidwe ati a umunthu watsopano amene apezeka pa Akolose 3 : 10 - 14 ? Nayenso Paulo anaona Ayuda monga ‘ anthu a mtundu wake [ “ monga mwa thupi , ” Buku Lopatulika ] . ’ — Aroma 1 : 3 ; 9 : 3 . ( Yobu 32 : 7 ) Mtumwi Paulo analangiza akazi acikulile acikristu kuti azilimbikitsa ena mwa mau ndi zocita . Kodi Yehova amapeleka citsanzo canji poseŵenzetsa ufulu wake ? Kodi lembali litanthauza kuti Yehova amaona zinthu zonse zabwino zimene munthu amacitila anthu ovutika ? Iye anati : “ N’nali kucita manyazi ndi mantha kukamba ndi anthu acilendo . Timayamba kuyamikila cilango ngati taona mapindu ake . Ndipo mapindu amene timapeza amaonetsa kuti Mulungu amatikonda . Timatsatila citsogozo ca Khiristu woukitsidwa amene nayenso amatsatila citsogozo ca Atate ake , Yehova . — Mat . Ndinali kuseŵenzela ku cipatala . Ngakhale kuti simumadya zizindikilo za pa Cikumbutso , mumapezekapo n’colinga coonetsa kuti mumayamikila nsembe ya dipo ya Yesu Kristu . Ndipo ena anali kumenyedwa koopsa ndi kuzunzidwa . Ngati ndinu wacinyamata , muli ndi mwai wamtengo wapatali wopanga mbili yabwino mwa kuika Yehova Mulungu pamalo oyamba , ndiponso mwa kucitila ena zabwino ndi kuwalemekeza . 4 : 6 ) M’nkhani ino , tikambilana mmene tingakhalile aphunzitsi aluso mwa ( 1 ) kufunsa mafunso kuti tidziŵe maganizo a mwininyumba , ( 2 ) kukambitsilana zimene Malemba amanena , ndi ( 3 ) kugwilitsila nchito mafanizo kuti timveketse mfundo . FUNSANI MAFUNSO KUTI MUDZIŴE MAGANIZO A MWININYUMBA Iye analolela kufa mozunzika pa mtengo wozunzikilapo pofuna kuti anthu ambili akapeze moyo . Ameneyu ndiye wokana Kristu , amene amakana Atate ndi Mwana . ” — 1 Yohane 2 : 18 , 19 , 22 . 10 , 11 ) Kucita zimenezi , kumathandiza kuti cilango cimene Yehova wapatsa munthuyo kudzela mwa akulu cigwile nchito bwino . “ Ndipo kumwamba kunabuka nkhondo : Mikayeli [ Yesu Khiristu ] ndi angelo ake anamenyana ndi cinjoka . Cinjokaco ndi angelo ake cinamenya nkhondo , koma sicinapambane , ndipo malo awo sanapezekenso kumwamba . Paulo anadzionela yekha mmene zimavutila kulimbana ndi zilakolako na zofooka za thupi lopanda ungwilo . 38 : 10 - 12 , 14 - 16 ) Mwa kuona kwa munthu , tidzaoneka ngati anthu opanda citetezo . Ngakhale n’telo , iye akumbukila bwino cinyengo ca abusa amene anali kuledzela , kuchova njuga , ndi kuba ndalama za m’mbale ya zopeleka kwinaku akumuphunzitsa kuti ngati wacimwa adzaochedwa ku moto wa helo . Iye anachula liu lililonse molondola ndipo sanalumphe mau alionse . n’ciyembekezo cokondweletsa cotani nanga cimene Baibo imatipatsa — Paradaiso wamuyaya ! Zimenezo zidzatithandiza kumvetsa zinthu . Conco , zolinga zanga zinasintha . Mukakhala bwenzi la ana anu ndi kuwathandiza kukhala bwenzi la Yehova , sizitanthauza kuti mwadzicotsela ulemu monga kholo . Mwina mungamuuzenso zimene mwakumana nazo mu utumiki . Conco , tiyeni tiyesetse kutengela cikhulupililo ndi kumvela kwa Nowa , Danieli , na Yobu . MADALITSO AMENE TIKUYEMBEKEZELA MU UFUMU WA MESIYA Citsanzo ca Mariya ciyenela kutilimbikitsa kuganizila zimene tingacite , kuti tionetse kuti timaika cifunilo ca Mulungu patsogolo mu umoyo wathu . Mwacitsanzo , kodi timacita bwanji ngati mbali ina ya m’Baibulo sigwilizana ndi zocitika za paumoyo wathu ? Monga oimila Watch Tower Society , M’bale Rutherford , Van Amburgh , na abale ena 6 anamangidwa . Mfundo imene Yesu anali kukamba apa ni yakuti : “ Ngati Mulungu amaveka cotelo zomela zakuchile . . . , kodi iye sadzakuvekani kuposa pamenepo , acikhulupililo cocepa inu ? ” ( a ) N’ziphunzitso zofunika kwambili ziti zimene zatithandiza kumvetsa uthenga wa m’Baibo ? Mau ake amati “ imfa sidzakhalaponso . ” Lefèvre d’Étaples ( womasulila ) , Na . Ndiye cifukwa cake nimapemphelabe kwa Mulungu za vutoli . ” Kodi ndine wofunitsitsa kudzimana zinthu zina kuti ndipeze coonadi , kapena ndimalola zinthu zina monga nchito yanga kundilepheletsa kupeza coonadi ? ’ ( Mat . 6 : 22 - 24 , 33 ; Luka 5 : 27 , 28 ; Afil . Iye anaitaniwa kuti akacite nawo maseŵela a Olympic , koma anakana . “ Muzitsanzila Mulungu , monga ana ake okondedwa . ” — AEF . Conco , abale acinyamata ayenela kuwathandiza . ( 1 Yoh . 2 : 16 ) Koma ise anthu a Yehova , timalimbikitsidwa kuti tiyenela “ kukana moyo wosaopa Mulungu ndi zilakolako za dziko , koma kukhala amaganizo abwino , acilungamo ndi odzipeleka kwa Mulungu m’nthawi ino . ” Phunzilani kuonetsa anthu cidwi mwa kuwafunsa mafunso mosamala kuti afotokoze maganizo awo , ndipo muziwamvetsela . Mwa kugwilitsila nchito mzimu wake , Yehova analemba Baibulo limene limatiuza makhalidwe ake abwino ndi cifunilo cake . Palibe mphatso ina yaikulu imene tinalandilapo kuposa imeneyi . N’cifukwa ciani Yesu anafotokoza fanizo la wofesa mbewu amene amagona ? Kodi mau a Yesu angakuthandizeni bwanji ? Kukumbukila lamuloli kudzatilimbikitsa kuonetsa cifundo ngakhale pamene zinthu zili zovuta . — Mat . Pokamba na akulu a mu mpingo wa ku Efeso , Paulo anaonetsa kuti kulimbikitsa ena na mau cabe , nthawi zina sikukhala kokwanila . Iye anawauza kuti : “ Muthandize ofookawo , ndipo muzikumbukila mau a Ambuye Yesu . N’zoona kuti mbali zina za m’Baibulo anazilembela anthu ena kapena gulu lina lake . Conco lamulani kuti akhwimitse citetezo pamandapo kufikila tsiku lacitatu , kuti ophunzila ake asabwele kudzamuba ndi kuuza anthu kuti , ‘ Anauka kwa akufa ! ’ Yehova anawasamalilanso mwakuthupi . Paulo anafotokoza kuti : “ Kuyesedwa olungama cifukwa ca kukoma mtima kwake kwakukulu kumene [ Mulungu ] wakusonyeza , powamasula ndi dipo lolipilidwa ndi Khristu Yesu , kuli ngati mphatso yaulele . ” — Aroma 3 : 23 , 24 . 12 : 21 - 24 . ( Chivumbulutso 4 : 11 ) Tikakhala okhulupilika kwa Yehova , timakhala osangalala ndi okhutila . Nkhawa zonse na kuvutika maganizo zidzaiŵalika . — Yesaya 65 : 17 . Ndipo cofunika kwambili ndi kudzifunsa kuti , ‘ kodi ndikucita zinthu mogwilizana ndi pemphelo limeneli ? ’ ( Chiv . 16 : 14 - 16 ; 19 : 19 - 21 ) Pomaliza , Mfumu Yankhondo idzapambana pa nkhondo yolimbana ndi adani ake mwa kuponya Satana ndi ziŵanda zake kuphompho kumene sadzatha kucita ciliconse . — Chiv . Komanso mungacite ciani kuti muzilalikila mogwila mtima ? 19 : 1 , 3 , 14 ) Atate wathu wacikondi amatidziŵa bwino kwambili . Nayenso Adamu m’malo momvela Mulungu , analandila cipatso kwa Hava . — Chiv . Ananditengelanso kwa abwana ao amene anandiuza kuti zipembedzo zonse n’zacabecabe . Hezekiya anamvetsela mwachelu malangizo ndi uphungu umene aneneliwo anam’patsa . ( Luka 21 : 21 ) Kodi io akanatuluka bwanji mu Yerusalemu popeza asilikali ambilimbili anali atazungulila mzindawo ? Yesaya 32 : 1 , 17 ; 54 : 13 Mwezi usanathe , ndinaganiza zoleka kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza bongo ndi kumwa moŵa . Khalani ndi colinga cothandiza ana anu kukonda Mulungu . ( Luka 22 : 25 , 26 ) Ndipo anawacenjeza kuti : “ Cenjelani ndi alembi amene amakonda kuyendayenda atavala mikanjo ndi kupatsidwa moni m’misika . ” — Maliko 12 : 38 . Molimba mtima , mtumwiyo anayankha kuti : “ M’dzina la Yesu Kristu Mnazareti uja , amene inu munam’pacika pamtengo , koma amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa , kudzela mwa iyeyo , munthu uyu waimilila pamaso panu atacila bwinobwino . ” — Mac . 4 : 5 - 10 . ( Maliko 13 : 19 ; Chivumbulutso 7 : 1 - 3 ) Panthawiyo , tidzafunika kumvela malangizo akuti : “ Inu anthu anga , pitani mukalowe m’zipinda zanu zamkati ndipo mukatseke zitseko . Yesu anabadwa patapita zaka zambili kucokela pamene Abulahamu anafa . Iwo adzakhala ngati manyowa panthaka . ’ ” ( Yer . Aramagedo ni malo ophiphilitsa oimila “ nkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu Wamphamvuyonse . ” Nkhondo yowononga anthu oipa . — Chivumbulutso 16 : 14 , 16 . “ Wodala ndi mtundu umene Mulungu wawo ndi Yehova , anthu amene iye wawasankha kukhala colowa cake . ” — SAL . Tiyeni tikambilane mmene makhalidwe amenewa angatithandizile kukhala okhulupilika kwa Yehova . 8 : 22 , 30 ) Sitingakwanitse kufotokoza mmene Yehova cinamuwaŵila panthawiyo . — Yoh . 5 : 20 ; 10 : 17 . Khalidwe lalikulu la Yehova ndi cikondi . Mosayembekezela , aliyense wa ife angakumane ndi nkhani yokhudza magazi . Msonkhano wacigawo ku Nyzhnya Apsha , Ukraine , 2012 Pali Ciyembekezo Cotani Ponena za Makolo Akale ? Ena amatumikila pa ofesi ya nthambi . Ndipo ena amathandiza kumanga maofesi a nthambi , maofesi omasulila mabuku , Nyumba za Misonkhano , kapena Nyumba za Ufumu . Kuti Timoteyo apewe zilakolako zimenezi , anafunikila ‘ kuzithaŵa . ’ Nthawi zina , anali kukhala m’dziko lacilendo , ndipo nthawi zinanso anali kukhala m’mapanga kucipululu . Kodi cizoloŵezi canga ca kuŵelenga , kavalidwe na kudzikongoletsa kwanga , kapena zimene nimacita nikapatsidwa uphungu zimaonetsa kuti ndine munthu wotani ? Iwo sanali kufunika kugwilitsila nchito ziphaso monga mapasipoti , kuti aloŵe m’dziko lina . Mwacitsanzo , kapepala kakuti , Kodi Ndani Maka - maka Amene Akulamulila Dzikoli ? , kamatsogolela m’phunzilo 5 la m’kabuku kauthenga . Ngati n’conco , tidzapewa cizoloŵezi cocita zinthu mongotsatila zimene takhala tikucita m’mbuyomu . Mosiyana ndi anthu amenewa , Aisiraeli a fuko la Zebuloni ndi la Nafitali “ anatonza miyoyo yawo mpaka kuiika pangozi , ” pothandiza Debora ndi Baraki . ( Ower . Cilamulo ca Mose cinali na malangizo omveka bwino a mmene Aisiraeli anafunika kusamalila ziwiyazo , ndipo aliyense wophwanya malangizowo anali kuphedwa . Conco , ciphunzitso cacikunja cakuti mzimu sukufa cinaloŵa mu “ Cikhristu , ” ndipo cinakhala mbali yaikulu ya zikhulupililo za machechi . Kodi Mkhristu amene ali kale na cimwemwe angathe kucikulitsa ? Kodi anansi ao angakuoneni bwanji ? Pambuyo pa kupanduka kwa mu Edeni , anthu apitilizabe kusamvela Mulungu . M’zaka zaposacedwapa , makhalidwe a anthu aipa kwambili kuposa kale . Lemba la Salimo 37 : 11 limati , ‘ Tidzasangalala ndi mtendele woculuka . ’ Kodi mau anga poyamikila ena ndi cikondi cimene ndimaonetsa , zimacokela pansi pa mtima ? — Sal . Anthu amene amapilila masautso adzalandila mphoto yotani ? Anauika pa gulaye ndi kuzungulutsa gulayeyo mofulumila pamwamba pa mutu wake . Cimene cionetsa zimenezi ni mau amene anauza abale ake . Kucokela nthawiyo , ndinasiya kukambilana ndi Mboni za Yehova . Abale kumeneko amayankha mafunso ambili pa nkhani zacisinsi na zovuta , zocokela ku mabungwe a akulu na oyang’anila madela a m’dziko lonse la United States . 11 : 40 ; Sal . Kuyambila mu 1939 , pacikuto ca Nsanja ya Mlonda pamakhala mau akuti “ Imalengeza Ufumu wa Yehova . ” ( 2 Timoteyo 1 : 6 ) Ganizilani anthu a m’gawo lanu ndiponso zimene mungakambe kuti akhale ndi cidwi . Mau a Ciheberi pa mavesiwa angamasulidwe m’njila zonse ziŵilizi . 1 : 5 ) Tifunikanso kuika ena patsogolo pathu . M’mipingo yambili , cangu ca mu ulaliki cinali citacepa ndipo utumiki wawo unali pamodzi - mpamodzi . Kodi tingati Abimeleki ndi Petulo anacita zinthu cifukwa ca mzimu wodzikweza ? Atacoka ku jele , anapita ku Hemsworth kukatumikila pamodzi na mng’ono wake Dennis , amene anali mpainiya wapadela . Robert Luccioni Anali mtumiki wa Abulahamu , m’bale wa agogo ake a Rabeka . ( a ) N’ciani cingalepheletse ena kuimba mokweza na mokondwela pamisonkhano ya mpingo ndiponso ikulu - ikulu ? Nanga tikanadziŵa bwanji za dipo ndi kuti Yehova amatikoka kupyolela mwa Yesu ? Ndinalibe nazo nchito kuti kaya anthu akukhudzidwa bwanji ndi zocita zanga . M’malo mwake , iye amatidalila kuti tidzakhalabe wokhulupilika ndipo amafuna kutithandiza . Nthawi zonse , tiyenela kuganizila mfundo yolimbikitsa ya pa Aheberi 11 : 6 , kuti Mulungu atiyanje ndi kutidalitsa . Nanga ali ndi makhalidwe abwanji ? Popeza ndinali ndi ngongole za njunga zoculuka kuposa pa $ 50,000 ndinapangana ndi anzanga aŵili kuti tikabe ndalama n’colinga cakuti ndibweze ngongolezo . Kuti mudziŵe cifukwa cimene Mulungu amalolela mavuto kucitika , onani nkhani 11 , m’buku ili , Zimene Baibulo Ingatiphunzitse , lofalitsidwa na Mboni za Yehova ] Komanso pambuyo pake , mkazi wake anamwalila ali na zaka 43 cabe . Tidzapitilizabe kupemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele mpaka iye atapambana pa nkhondo yake ndi kucotsa zoipa zonse zimene zikucitika padziko lapansi . Koma zimenezo si zoona . Mwacitsanzo , nthawi zina anthu a m’banja lanu angakuletseni kupita ku misonkhano yampingo kapena yadela . Amidiyani anapondeleza Aisiraeli kwa zaka zambili moti Gidiyoni ndi asilikali ake anaona kuti afunika kuwagonjetsa basi . Nanga n’ciani cimene cingacitike ngati dzila latuluka ndi kulumikizana na mbeu ya mwamuna ? Na ise timacita cidwi kuona kuti maulosi a m’Baibo amenewa okamba za kuuka kwa Yesu anakwanilitsika , ngakhale kuti panapita zaka zambili kuti zimenezi zicitike . Ndinali nditangocoka kucipatala kumene ndinali kuseŵenza . 2 : 2 ) Iyai . Angelo ndi apamwamba kwambili kuposa anthu . Adilesi ya Webusaiti yathu ndi www.jw.org . Ngakhale zithunzi zimene n’najambula zinali kuonetsa nkhawa zanga . Na ise sitingadziŵe madalitso onse amene Yehova adzatipatsa m’tsogolo . 12 : 20 ) Ngakhale pamene anakumana na zinthu zokhumudwitsa , Yesu anali kucita zinthu mokoma mtima ndi mwacikondi . TSAMBA 16 Izi zinanithandiza kumvetsetsa coonadi . Amaphunzila mmene angalalikilile kwa anthu amene sadziŵa Baibo na mmene angayankhile pa misonkhano ya mpingo . Amakhalanso otangwanika na zocita zina zambili zotsitsimula mwauzimu . ” Popeza kuti amai a mnyamatayo anayankha modekha ndi mokoma mtima , alongowo anakhalabe mabwenzi . Manje funso n’lakuti , Kodi tingapeze bwanji nzelu zopindulitsa na kuzisunga ? Nanga tidziŵa bwanji ? Pamene Mose anali mwana , amai ake a Yokebedi , anam’phunzitsa za Mulungu wa Aheberi . Mu 1993 , n’nabatizika kukhala wa Mboni za Yehova , ndipo mu 2000 n’nakwatila Tabitha , mtumiki mnzanga wokangalika . Koma mau alionse ouzilidwa amene amatsutsa zoti Yesu anabwela monga munthu , amenewo si ocokela kwa Mulungu , ndipo ndi ouzilidwa ndi wokana Kristu amene munamva kuti akubwela , ndipo tsopano ali kale m’dziko . ” Pulofesa wina wa chemistry anati : “ Kuti moyo upitilize pamafunikila ( 1 ) cibelekelo , ( 2 ) mphamvu ya moyo , ( 3 ) malangizo a m’majini , ndi ( 4 ) mphamvu yokopela malangizo a m’majiniwo . Tinali kukhala m’nyumba za abale . Ngakhale kuti nyumbazo sizinali zapamwamba , zinali zaudongo nthawi zonse . Kafuku - fuku wina amene anacitika ku America , anaonetsa kuti 78 pelesenti ya akulu - akulu olemba anthu nchito m’makampani , anakamba kuti kukhulupilika ni “ cimodzi mwa zinthu zitatu zofunika kwambili kuti munthu aloŵe nchito . ” Koma funso lofunika kwambili ndi lakuti : Ndi liti pamene nthawi zokwanila 7 zinatha ? 28 Kukhalabe Bwenzi Pakacitika Zinthu Zimene Zingasokoneze Ubwenzi Mafilimu , mabuku , nyimbo , ndi zinthu zina zotsatsa malonda zimalimbikitsa khalidwe laciwelewele . Zimene tinaona pa msonkhano wacigawo wa ku Dublin nthawi zonse zizitikumbutsa mwai wamtengo wapatali umene tili nao wotumikila Mulungu wathu wamkulu limodzi ndi inu nonse . ” MABWENZI AMAKAMBILANA Iye anasankha anthu amene anali kuopa Mulungu , okhulupilika , ndi odalilika . Mudzapezapo mabuku ambili kuphatikizapo otsatilawa : Ndipo anthu anamva bwanji atalilandila ? A Mboni za Yehova salosela za kuonongeka kwa dziko . Mtumwi Paulo analemba kuti “ Mulungu amakonda munthu wopeleka mokondwela . ” Zikomo pondipatsa mwayi wocita zopeleka . Izi zimanicititsa kumva bwino . ” Muziunika mfundo zofunika pa lemba ndi kuzifotokoza ( Mat . 13 : 22 ) Anthu ambili amaganiza kuti ndalama ndiponso zinthu zina zakuthupi zingawapatse cimwemwe . Mkango wanjala sucita cifundo ukafuna kugwila nyama , kapena pambuyo pogwila nyamayo . Mfundo imene sitiyenela kuiŵala ndi yakuti : Sitimatsutsa ngati Malemba akamba kuti munthu winawake , cocitika cinacake , kapena cinthu cinacake , cimaimila cinthu cina mtsogolo . Tsopano ndili ndi zaka 43 , koma ndine wamfupi mita imodzi . 18 : 12 - 14 ; Luka 12 : 6 , 7 . NYIMBO : 94 , 134 Iye anapitilizabe kukhulupilila Mulungu , kukhala wokoma mtima , wodzicepetsa , ndiponso wopilila . Pa cifukwa cimeneci Yehova anamudalitsa panthawi yake . Cikhulupililo n’cofunika kwambili . Palibe mdani aliyense anapulumuka nkhondo imeneyo . — 2 Mbiri 14 : 11 - 13 . Kuti tithandize abale ndi alongo athu , tiyenela kuwadziŵa bwino coyamba . Tutakula , ndinatugulitsa ndipo ndinagula twina toposa 300 . Kale , n’nali kudziona ngati munthu wopanda pake , koma tsopano nimadzilemekeza ndipo nili na mtendele wa m’maganizo . Yehova anatilenganso m’njila yakuti tizisangalala ndi zosangulutsa ndiponso kupindula nazo . Pemphelo lake lokhudza mtima limapezeka m’Baibo . Mfumu Asa anaonetsa cangu kwambili pakulambila koona pamene anacotsa mahule a pakacisi . Ndipo anathetsa kulambila mafano kumene kunali kofala m’dzikolo . Ha , ndife okondwa cotani nanga pa madalitso onsewa ! Tingaphunzilepo ciani pa zozizwitsa za Yesu ? Wadela wina anati : “ Nthawi zina abale na alongo amatilembela makalata otiyamikila . Amakamba mmene asangalalila pa kucezetsa kwathu . Posacedwa , Christine anamanga banja ndi Gideon , ndipo atumikila pamodzi ku Ghana . Magazini ya The Watch Tower ya October 15 , 1923 , inakamba kuti “ Mwana wa munthu ” ndi Yesu . Masiku ano , anthu ambili ali ndi Baibulo ndipo zimenezi zimatithandiza kuwaphunzitsa uthenga wabwino . Pa nkhani imeneyi , Mulungu anali atamulamula kuti asatsatile milungu ina , koma iye sanasunge zimene Yehova analamula . ” Kodi “ kuika maganizo pa zinthu za thupi ” kusiyana bwanji na “ kuika maganizo pa zinthu za mzimu ” ? Cifukwa cakuti tikhoza kuphunzilapo kanthu pa zitsanzo za anthu opanda ungwilo amenewa amene anakanganapo ndi anthu ena . Cifukwa cakuti tikamalalikila , timaonetsa kuti tikukhulupilila kuti mapeto ali pafupi , ndiponso kuti “ sadzacedwa . ” Pozindikila mfundo imeneyi , Yesu anakamba kuti : “ Osaukawo muli nawo nthawi zonse . ” Baibulo limafotokoza ziyeneletso zina zimene akulu ayenela kukwanilitsa . Kwa kanthawi , abale amenewa analibe ufulu wocita zinthu zauzimu . Koma patapita zaka , mwanayo anamwalila . Ku South Africa ( b ) Fotokozani citsanzo . Mu Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso la 2013 , dzina la Mulungu limapezekamo nthawi zokwana 7,216 . Mulungu anaonetsetsa kuti mau na zocita zake zalembedwa m’Baibo . Munthu aliyense amene amakondadi Yehova ndipo amafuna kukhala wokhulupilika kwa iye , “ akalumbila kucita zinthu zimene kenako zakhala zoipa kwa iye , sasintha malingalilo ake . ” Tili ndi citsanzo cabwino kwambili ca ana a Nowa . Onani zitsanzo izi . ( Neh . 13 : 23 - 26 ) Conco , pofuna kuti atumiki ake zinthu ziziwayendela bwino , Mulungu watipatsa malangizo akuti tiyenela kukwatila olambila oona . ( Sal . 19 : 7 - 10 ; Yes . Mtumwi Paulo anafotokoza cifukwa cake m’mau awa akuti : ‘ Ucimo unaloŵa m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi , ndi imfa kudzela mwa ucimo , imfayo inafalikila kwa anthu onse . ’ N’zokondweletsa kuona kuti mwayi woloŵa masukulu ophunzitsa atumiki a Mulungu ukuwonjezeka . Nimayamikila kwambili mwayi woonana ndi abale ndi alongo ambili amene amadzipeleka kukalandila maphunzilo amenewa . Tsopano tiyeni tikambilane mitundu iŵili ya masautso amene tingakumane nao . M’kupita kwa nthawi , cisotico cinathandiza anthu ‘ kukumbukila ’ zimene iwo anacita pocilikiza kulambila koona . Komabe , Baibo imakamba kuti : “ Munthu wokonda siliva sakhutila ndi siliva , ndipo wokonda cuma sakhutila ndi phindu limene amapeza . ” Mudzaona kuti Baibulo si buku lovuta kumvetsetsa , koma ‘ ndi lopindulitsa pa kuphunzitsa , kudzudzula , kuongola zinthu ndi kulangiza m’cilungamo , kuti munthu wa Mulungu akhale woyenelela bwino ndi wokonzeka mokwanila kucita nchito iliyonse yabwino . ’ — 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 . Ndinamangidwa kambilimbili , ndipo kwa zaka zambili ndimangoloŵa ndi kutuluka m’ndende . Koma lipoti ya mu 2013 , inaonetsa kuti caka ciliconse anthu 9 miliyoni a zaka zosakwana 60 , amafa na matenda a mtima , sitroko , khansa , matenda a m’cifuwa , ndi a shuga . Komabe , kaya ndife acinyamata kapena acikulile , ndiponso mosasamala kanthu za kumene tinakulila , Mulungu amafuna kuti tizimulambila mogwilizana . 5 : 6 , 7 ) Kucita zinthu modzicepetsa , kudzakuthandizani kupeza ciyanjo ca Mulungu ndi thandizo lake . Abele , Enoki , Nowa , Abulahamu , ndi anthu ena ngati amenewa anali kukhulupilila kuti akufa adzauka . Ndani angakupatseni malangizo abwino kwambili okhudza nchito ? Kunena zoona , tonse tiyenela kuyembekezela kukumana ndi mavuto polalikila uthenga wa Mulungu wopatsa moyo wa coonadi m’dziko limene likulamulidwa ndi “ woipayo , ” amene ndi Satana Mdyelekezi . — 1Yoh . Kodi mukuthandiza ana anu kucita zinthu mogwilizana ndi pempho lakuti cifunilo ca Mulungu cicitike pa dziko lapansi ? ( Oweruza 11 : 4 - 11 ) N’ciani cinathandiza Yefita kucita zinthu mwa njila imeneyi ? Coyamba , tikuuzidwa kuti mboni zimenezi “ zikuimilidwa ndi mitengo iŵili ya maolivi , ndi zoikapo nyale ziŵili . ” ( Chiv . Kukhwima sikutanthauza cabe kukula kwa msinkhu kapena kuculuka kwa zaka zimene munthu ali nazo . Palibe buku lina lakale limene lili ndi mipukutu yambili imene inalembedwa kale kwambili monga ya Baibulo . Apainiya apadela ambili amathela maola 130 mu ulaliki mwezi uliwonse . Kodi mungamuthandize bwanji munthu amene asamalila makolo okalamba ? Nanga adzaukitsidwila kuti ? 3 : 7 ) Timabyala ndi kuthilila , koma sindife amene timakulitsa . Ndalankhula kwa Koresi amene ndamugwila dzanja lake lamanja kuti ndigonjetse mitundu ya anthu pamaso pake , kuti ndimasule m’ciuno mwa mafumu , kuti ndimutsegulile zitseko zokhala ziwiliziwili , moti ngakhale zipata sizidzatsekedwa . ” 11 : 6 , 11 - 13 . Ngakhale pamene muli na nkhawa yaikulu , Yehova angakuthandizeni kukhala na mtendele wa mu mtima . Timafunika kukonda anzathu mmene timadzikondela . Nthawi zambili , makolo awo na amene amawauza kuti asabatizike mwamsanga . Koma ophunzila a Yesu cinawavuta kukhulupilila zimenezi cifukwa anali ndi cikhulupililo cocepa . ( Mat . Cinanso , pamene muceza na abale na alongo , bwanji osawafunsako mmene kukoma mtima na khalidwe lawo labwino zakhudzila abululu awo , maneba , anzawo a kunchito , kapena a kusukulu ? Nzelu ndi limodzi mwa makhalidwe akuluakulu a Yehova , ndipo iye akafuna amaonelatu zinthu zamtsogolo . Ni mafunso ati amene tingafunse okhudza kuuka kwa akufa ? Tili ku Puerto Rico , tinali kupita ku England kukaona makolo nthawi zambili . “ Ndiwe Mkazi Wokongola m’Maonekedwe Ako ” Pokambilana ndi ena , uziseŵenzetsa zida zimene zilipo m’cinenelo canu ( Onani ndime 5 ) Mwina mufunika kuongolela mmene mumaphunzilila Baibulo . ( Ŵelengani Luka 22 : 28 - 30 . ) Yesu anakamba kuti tiyenela kulambila Mulungu m’coonadi . Coonadi cimeneci cipezeka m’Baibulo . 16 - 18 . Koma musalole kuti Satana akunyengeleleni mwa njila imeneyi . ( Mateyu 11 : 28 , 29 ) Nthawi zambili , iye anali kuthetsa mavuto ao ndiponso kuwathandiza kukhala pa ubwenzi wabwino ndi Yehova . Koma m’kupita kwa nthawi , tinamulola kupita ndipo tinacita bwino kwambili . ( Yer . 31 : 3 ; 2 Akor . Ndipo cifukwa cakuti sadziŵa uthenga wa Yesu , samvetsetsa cifukwa cake ayenela kulalikila . Pambuyo pake , ndinazindikila kuti tinali ndi zolinga zofanana . ( Mat . 6 : 24 ) Ngati tikhala kapolo wa Cuma , tikhoza kusiya kutumikila Yehova , ndipo zimenezo n’zimene Satana amafuna . ya October 8 , 2003 . Ndani sangafune kuyandikila munthu wotelo ? Yehova adziŵa kuti tikapitiliza kuphunzila za iye m’Baibulo , iye adzakhala weniweni kwa ife , ndipo tidzamuyandikila kwambili . Kodi nimalolela kudzimana zosangalatsa zina pofuna kutumikila Mulungu ? Pophunzila cineneloci tinali kugwilitsila nchito matepu . Komabe , kaya tili m’cikwati kapena ai , tonse ‘ tingavule colemela ciliconse ’ cimene cingatisokoneze potumikila Yehova . Conco , tiyenela kucititsa eninyumba kukhala omasuka . ( Afil . Mabuku athu akhala akutilimbikitsa kuti tiyenela ‘ kuyembekezela ndi kukumbukila nthawi zonse kukhalapo kwa tsiku la Yehova . ’ 3 : 9 ; 11 : 25 . Ngati uona kuti sungakwanitse kufotokoza bwino - bwino za cisanduliko kapena za cilengedwe , ungayese njila yosavuta imene Paulo anaseŵenzetsa . Nanga cofunika makamaka n’ciani ? ” Tingacite ciani kuti tilimbitse mgwilizano pakati pa anthu a Mulungu masiku ano ? Mwakutelo , mudzakhala mukutamanda Atate wathu wakumwamba monga mmene Davide anacitila : Iye anaimba kuti : “ Ndidzatamanda Yehova nthawi zonse . Ndipo zinthu zitafika poipa , iye anam’thaŵa mkaziyo . M’kupita kwa nthawi , anthu 30 a m’banja lina limene tinaphunzila nalo Baibo anakhala Mboni . Pamene anali kukambitsilana ndi mkazi wina pabwalo la nyumba yake , mvula inayamba kugwa . 4 , 5 . ( a ) Ni cilimbikitso canji cimene Yehova anapeleka kwa anthu ake akale ? Khalani ndi Mzimu Wodzimana , 3 / 1 Patapita nthawi , n’nadziŵa kuti M’bale Knorr anali kuthela nthawi yoculuka kuŵelengela zofalitsa M’bale Franz cifukwa ca vuto lake la maso . Tiyeni tikambilaneko mfundo zinayi zimene zingacititse kuti wolandila mphatso asangalale nayo . Nyimbo zina ‘ zimatilimbikitsa pa cikondi ndi nchito zabwino . ’ Tingacitenji kuti tidziŵe ngati timakondetsetsa cuma ? ( Mlaliki 3 : 11 ) Timafuna kusangalala ndi moyo padziko lapansi lokongola kosatha , osati cabe kwa zaka 80 kapena kuposelapo . Zimenezi zinam’dabwitsa Fernando , ndipo anafunsa kuti , “ Mwati bwanji ? ” Cifukwa ca cikhulupililo cawo , aneneli monga Mikaya na Yeremiya ‘ analandila mayeselo awo mwa kutonzedwa . . . ndi [ kuikidwa ] m’ndende . ’ Kukhala Mkristu wokhulupilika n’kwabwino kwambili kuposa kukondedwa ndi anthu amene satsatila malamulo a Yehova . Pakufunikanso abale ena amene angakwanitse kupita kukathandiza nchito yomanga ku maiko ena . COLINGA : Kuteteza “ mbeu ” ndi kuthandiza anthu kudziŵa Mesiya N’ciani cingatithandize kuona zinthu zimene Mulungu amaticitila ? Umboni ni wakuti Yobu anali atafa kale - kale pamene Ezekieli anali kulemba mau a mu lemba la mfundo yaikulu ya nkhani ino . Maboma amenewa adzaloŵedwa m’malo ndi “ kumwamba kwatsopano ndi dziko lapansi latsopano ” kutanthauza Ufumu wa Mulungu umene ndi boma lakumwamba lolamulila anthu okhala pa dziko lapansi latsopano . — Chivumbulutso 21 : 1 . 9 , 10 . ( a ) Kodi Nyumba za Ufumu zatsopano zimamangidwa bwanji ? Nanga zotsatila zake zakhala zotani ? Koma kodi Davide , amene anali wacicepele panthawiyo , anacita ciani ? Izi zimatithandiza kupeza vesi m’Baibulo mosavuta . Kucita zimenezo n’kofunika kuti tipitilizebe kukhala oyela . ( Miyambo 3 : 27 ) Conco kugwila nchito mwamphamvu kungatithandize kukhala wosangalala kwambili ngati timathandizanso ena . Mwa kucita izi , ndiye kuti mukukhomeleza mfundozo m’maganizo mwanu na kuziseŵenzetsa pothandiza ena . Nthawi zina , sitinali kumvela bwino mumtima tikamvela ana athu akukamba kuti sakhulupilila mfundo zina za coonadi . Ndi njila ina iti imene Yehova amaonetsela kuti amatikonda ? Yankho ikuti : “ Malemba aonetsa kuti sayenela kubatizika . ” Nanga zimene anawauzazo zinawakhudza bwanji ? 2 , 3 . ( a ) Kodi acinyamata acikristu ayenela kupewa ciani ? Mikangano . Mwacitsanzo , ngati timakonda kulakalaka zaciwelewele , tingacite zimene tikulakalazo mpata ukapezeka . Mosonkhezeledwa ndi mngelo wopanduka , amene anadzachedwa kuti Satana Mdyelekezi , Adamu ndi Hava , anakana kutsatila malamulo a Mulungu osiyanitsa cabwino ndi coipa mwa kudya “ zipatso za mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa . ” 5 : 28 , 29 ; 11 : 23 ) Potsimikizila kuti Yehova angathe kuukitsa akufa , Yesu pa nthawi ina anakamba kuti Abulahamu , Isaki , na Yakobo , ‘ onse ni amoyo ’ kwa Mulungu . ( Miy . 16 : 9 ) Koma tikasankha njila yolakwika tidzakumana ndi mavuto . Pulofesa wina dzina lake Moshe Goshen - Gottstein analemba kuti : “ Iwo anali kuona kuti kusintha mwadala mau a m’Baibulo ndi mlandu waukulu . ” Pamene Yosefe anatengedwa kuloŵela kum’mwela njila yopita ku Iguputo , anaoneka ngati watayika . Mwacitsanzo , mayi wina wochuka wa mafilimu anati : “ N’zosatheka kukhala ndi mwamuna kapena mkazi mmodzi . N’cifukwa cake , Adamu ndi Hava atacimwa , Yehova anawalola kubala ana . Ife kwathu n’kukondwela kuti tinamasulidwa mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu . ( Aroma 12 : 12 ) Cinanso , masiku ano Yehova watipatsa gulu labwino la olambila anzathu . Kodi tiphunzilapo ciani pa colakwa cimene Asa anacita ? Mvelani mmene mkulu wina mumpingo wa ku Canada anaphunzilila kufunika kotulila Yehova nkhawa zake . Yehova samangouza ife anthu kuti tikhale oleza mtima , koma iyeyo watipatsa citsanzo cabwino kwambili pa nkhani imeneyi 13 : 34 , 35 . M’pomveka kuti Yesu anagogomeza kwambili kufunika kwa mgwilizano . M’dela la Kilkenny tinali kuphunzila Baibulo ndi m’nyamata wina katatu pa mlungu ngakhale kuti magulu a anthu aciwawa anali kutiwopseza . N’ciani cinam’thandiza kukhala wolimba conco ? Yesu anali kukamba kuti kumwamba ndi dziko lapansi zingacoke kusiyana n’kuti mbali yocepa kwambili ya m’Cilamulo isakwanilitsike . Iwo adzakhala ndi mwayi wokhala ndi moyo wosatha padziko lapansi . — Mateyu 25 : 34 , 46 . Ndipo munthu aliyense payekha ndi wapadela . Komabe , Gehazi , mtumiki wa Elisa , anakhumbila mphatso zimenezi . Mboni za Yehova sizimaona zamtsogolo , kumva mau ocokela ku mizimu kapena kulosela zamtsogolo . Yehova ndi mtetezi wabwino kwambili kuposa wina aliyense . — Mat . Cofunika ni kucita zopelekazo na colinga cabwino . ( Ŵelengani Mateyo 6 : 19 - 21 , 24 - 26 , 31 - 34 . ) Papita zaka 10 kucokela pamene tinaphunzila Cichaina . N’natumikila pa famu imeneyi kwa zaka pafupi - fupi zitatu . Conco , tiyeni ticite zilizonse zimene tingathe kuti tikonze cipulumutso cathu . Kuyambila m’caka ca 1949 , cifukwa ca zifukwa zina , abalewo analeka kugwilizana ndi gulu ndipo anakhazikitsa mipingo yao . Ali kumtenjeko , anapita pa malo ena owala bwino okhala na mawindo otsegula . Conco , ngati mlongo wayamikila m’bale pa khama lake , ndiye kuti zimene wakamba ndi zenizeni , ndipo ndi zimenenso abale okhwima kuuzimu angakambe . Iye anati : “ Ndinacita manyazi kwambili , koma nditapemphela kwa Yehova , ndinakhala ndi mtendele wa mumtima . ” Ngakhale kuti kusintha kumeneku kungacititse abale ndi alongo amene akutumikila panthambi zimenezo kupanga masinthidwe paumoyo wao , m’kupita kwa nthawi io amaona ubwino wake . ( Mlal . Tingasankhe bwanji mabwenzi abwino ? Hannah anati : “ Nthawi iliyonse tikatsiliza kuphunzila , pobwelela ku nyumba tikuchova njinga , tinali kuyang’anana ndi kukamba kuti : ‘ Zikomo Yehova ! ’ ” Koma akaphunzila coonadi , aliyense payekha amakhala na ufulu wodzisankhila amene afuna kum’tumikila . Conco , mwamsanga anabweza zonse kwa akulu a m’delalo monga mmene anazipezela . Ngakhale n’telo , ine ndi Maxine titaonananso ndi M’bale Knorr , anatipempha kupita ku nyumba kwake ndipo anatikonzela cakudya . Mwacitsanzo , ku Girisi , ngati munthu wamenya makolo ake , anali kulandidwa ufulu uliwonse umene anali nawo monga nzika . Ndipo m’malamulo a Aroma , kumenya tate unali mlandu waukulu kulingana na mlandu wa kupha munthu . Ndinagela tsitsi langa lalitali , kutaya masikiyo anga , ndi kusiya kutukwana . 30 : 8 , 20 - 24 . Onani Nsanja ya Olonda ya October 15 , 1999 , masamba 23 - 27 . Komabe , Paulo sanatanthauze kuti munthu ‘ akaika maganizo pa zinthu za thupi , ’ ndiye kuti basi mapeto ake ni imfa . Kodi pali aliyense amene anandiuzapo kuti ndisiye kum’tumila mauthenga ? ( Mat . 6 : 9 ) Mwacitsanzo , pamene tiuzako ena coonadi ponena za makhalidwe abwino a Yehova na colinga cake cosasinthika kwa anthu , timakhalila kumbuyo dzina la Mulungu potsutsa mabodza a Satana na zinenezo zake . ( Gen . Yehova amaona zonse zimene timacita ndipo adzatidalitsa . Yehova adzakutonthozani ndi kukupatsani mphamvu . Koma Akristu sayenela kukamba mau aukali kapena oipa , ngakhale moseka cabe . Izi zidzacitika pambuyo poti abale onse otsalila a Kristu amene adzakhala akali padziko lapansi adindidwa cidindo comaliza . ( Chiv . Colinga cathu povala umunthu watsopano cifunika kukhala kulemekeza Yehova , osati kuti anthu azititamanda . Pa Oweruza 5 : 9 , 10 , tionapo kusiyana kwina pakati pa anthu amene anadzipeleka kukamenya nkhondo na Baraki ndi amene sanadzipeleke . Ganizilani zifukwa ziŵili izi zofunika kwambili . Kodi Ndani Anapanga Mulungu ? Sept . Mofanana ndi Abulahamu , nafenso tiyembekezela kukwanilitsidwa kwa malonjezo a Mulungu . Lankhulani zoona m’khoti . Onse anali kutsatila citsanzo ca Mtsogoleli wao , Yesu Kristu . Mau a Mulungu amati pali “ nthawi yoseka . . . ndi nthawi yodumphadumpha mosangalala . ” ( Mlal . N’cifukwa ciani pempho la cakudya cathu calelo ndi lofunika ngakhale kuti tili ndi zinthu zokwanila za kuthupi ? Timasangalala ndi mwai wokhala anthu ocedwa ndi dzina lake ndiponso cifukwa cokhala Mboni zake . Pamene Yesu anali pa dziko lapansi , kodi Yehova anaonetsa bwanji kuti anali kumuyanja ? Ndi cocitika citi ca mtsogolo cimene cidzayesa cikhulupililo cathu ? Timalakalaka nthawi pamene ukalamba , kuvutika ndi kupanda ungwilo zidzatha . Conco , iye anaona kuti m’pofunika kuti adziteteze . 23 : 1 , 2 ; Rute 1 : 3 , 12 . Atafika zaka 14 , anayamba kucita upainiya , ndipo tinacitako pamodzi upainiya kwa zaka ziŵili . 15 : 4 ) Kukhala oona mtima kumatithandiza kukhalabe pa ubwenzi wabwino ndi Yehova . Zinthu paumwana wanga zinali zovuta kwambili . Kuti munthu amange nyumba mpaka kuimaliza amafunika kukonzekela bwino . Naonso acinyamata ayenela kukonzekela bwino akalibe kubatizidwa kuti atumikile Yehova mokhulupilika “ mpaka pa mapeto . ” ( Onani ndime 10 , 11 ) ( Yakobo 1 : 5 ) Mukhoza kucita zinthu mogwilizana na mapemphelo anu mwa kuŵelenga Baibo na kuseŵenzetsa zimene mwaphunzila . Nanga zimenezo ziphatikizapo ciani ? Kodi Yesu anafuna kuti ophunzila ake azicita ciani ? M’nkhani ino , tidzakambilana mmene zocita za ena zingatilepheletsele kuyang’anabe kwa Yehova . 14 : 8 - 19 . ( October 1 , 2010 ) ; “ Kodi Yesu Ndi Mulungu ? ” Uthenga waciweluzo umene Inoki analengeza ni cenjezo kwa anthu onse masiku ano monga mmene zinalili m’nthawi ya Inoki . M’kupita kwa nthawi , n’nazoloŵela kutamba zamalisece . Adamu na Hava asanafe cifukwa ca ucimo ndi kupanda ungwilo , anabala ana amuna ndi akazi . ( Gen . Onani nkhani yakuti “ Tengelani Citsanzo Cao ” m’magazini ya Nsanja ya Mlonda ya September - October 2014 . ZIMENE MAU A MULUNGU AMAPHUNZITSA : Yehova samangoona kupanda ungwilo kwanu , iye amadziŵa mmene inuyo mulili . Komabe , Akhristu amakhulupilila kwambili lonjezo la Yesu lakuti akufa adzauka . N’cifukwa ciani zimene Yesu anayankha Petulo n’zolimbitsa cikhulupililo ? Malemba amakamba cabe za anthu aŵili amene anakondwelela masiku awo akubadwa . Kapena tili cabe na zibadwa zosiyana ? ’ Nchito na Ndalama . — Miyambo 10 : 4;28 : 19 ; Aefeso 4 : 28 . Komanso , kukhala na cikondi kumaonetsa kuti tikutengela Yehova , Gwelo la cikondi . ( Aef . Akali kukamba , Yesu anaonekela kwa onsewo . Mau amenewa ni a mphamvu kwambili . Iye anati : “ Inuyo mwandisiya , conco inenso ndakusiyani ndipo ndakupelekani m’manja mwa Sisaki . ” Kodi mungaŵelenge zimene Yesu anakamba kothela kwa vesi loyamba ? 26 : 4 , 5 ; Afil . 3 : 4 - 6 ) Iye anakamba modzicepetsa kuti : “ Ndine wamng’ono kwambili mwa atumwi onse , ndipo si ine woyenela kuchedwa mtumwi . ” Mu 2001 , boma la Australia linasindikiza Buku limeneli ndi kupatsa anthu a ku Tuvalu monga mphatso . Cifukwa cakuti kudela nkhawa kwambili cifukwa ca zinthu zofunikila mu umoyo sikungacititse kuti tikhale moyo utali . 19 : 4 ; Yobu 7 : 7 ) Ngakhale zinali conco , iwo sanataye mtima , koma anadalila thandizo la Yehova . Koma analeka cifukwa cakuti anayamba kukonda Yehova ndipo anafuna kum’kondweletsa . Lemba la 1 Yohane 5 : 3 limafotokoza cifukwa cake cikondi n’cofunika . Kodi mphatso zimene anakamba ni ziti ? Nanga timapindula bwanji na mphatso zimenezi ? Mpingo wacikhiristu woyambilila nawonso unali wadongosolo . Ndipo unali kupindula ndi malangizo ocokela ku bungwe lolamulila . Kuwonjezela pa kukhala mnzanga , iye analinso citsanzo cabwino kwa ine pa zinthu zauzimu . ” Ganizilani za Hagara , mzimai waciiguputo wa m’zaka za m’ma 1900 B.C.E . M’malomwake , Yesu anatsimikizila Petulo ndi atumwi ena kuti amawadalila . Koma m’Baibulo muli mfundo zosavuta kumva zimene zimathandiza . Conco , nthawi zambili , iye ‘ amapeleka njila yopulumukila ’ mwa kutipatsa zimene tifunikila kuti tikwanitse kupilila mayeselowo . Madzulo tsiku limenelo ndinafunika kupita ku nchito . Tsopano , tiyeni tikambilane aŵili mwa makhalidwe oipa amene mtumwi Paulo anachula . Makhalidwewa ni dama komanso zinthu zodetsa . — Ŵelengani Akolose 3 : 5 - 9 . ( Luka 24 : 32 , 45 ) Yesu anali kukonda Mau a Mulungu , ndipo anali wofunitsitsa kuuzako ena . ( Luka 11 : 13 ) Kumbukilani kuti kufatsa na kudziletsa , zili mbali ya cipatso ca mzimu woyela wa Mulungu . Akristu aŵili odzicepetsa amenewa , anavutika kuletsa khamu la anthulo kupeleka nsembe kwa io . — Machitidwe 14 : 11 - 18 . Conco , dziikileni colinga cakuti muzikhala na “ zocita zambili nthawi zonse mu nchito ya Ambuye . ” — 1 Akor . ( Mateyu 24 : 21 ) Pambuyo pa cisautso cacikulu , tidzalandila malangizo atsopano amene tidzayenela kutsatila m’dziko latsopano limene simudzakhala Satana . Pambuyo pake , tinali kukhala na nchito yoyeletsa pulojekita . Koma pamene Baibo ikamba za kumwamba kweni - kweni , imatanthauza mumlengalenga , kumwamba kumene kuli nyenyezi , kapena malo okhala Mulungu . Zotulukapo zake zinali zakuti iye anakhala na cikhulupililo colimba . Cifukwa ndife opanda ungwilo , nthawi zina tonse timacita zinthu modzikuza . Kodi Aisiraeli anaonetsa bwanji kuti sanayamikile ufulu umene Yehova anawapatsa ? Mwacitsanzo , pa Ekisodo 34 : 6 , 7 , Yehova anauza Mose kuti iye ndi “ Mulungu wacifundo ndi wacisomo , wosakwiya msanga ndiponso wodzaza ndi kukoma mtima kosatha ndi coonadi . Koma pali odzozedwa ocepa cabe amene akali padziko lapansi , ndipo pali nchito yaikulu yofunika kucitidwa . Mwaphunzilanso mmene mungalimbikitsile madokotala kucita maopaleshoni popanda kugwilitsila nchito magazi . Iye ayenela kutengela citsanzo ca mmodzi wa aneneli akale . Cocitika Cimene Simuyenela Kuphonya Usiku wakuti maŵa apeleka moyo wake , Yesu anauza otsatila ake okhulupilika kuti azikumbukila imfa yake . Tiyenela kukhala osangalala podziŵa kuti Yehova adzatipatsa zinthu zambili zabwino m’Paladaiso . Kodi atumiki anthawi zonse amaona bwanji thandizo ndi cilimbikitso cimene ena amapeleka ? Iye anati : “ Imeneyi inali nthawi imene ndinatsimikizila kuti Yehova ndi weniweni ndipo amandikonda kwambili . ( a ) N’ndani amene ali pa ubwenzi wapadela na Yehova masiku ano ? Komanso nawonso acinyamata , afunika kukhala oleza mtima ngati sapatsidwa maudindo owonjezeleka . Paulo anapeleka citsanzo cabwino pankhaniyi . Iye anayamikila kwambili , ndipo analonjeza kuti adzamubwezela ndalama zoposa madola 20 . Anthu ayenela kuti anadabwa kwambili kuona iye akutenga cisotico n’kuveka Mkulu wa Ansembe , Yoswa . * Komabe , tingapindule kwambili ngati okonzanso Baibo angacite zimenezo cifukwa cokonda kwambili Mulungu . Anthu ena akakumana ndi vuto lotelo amayamba kudziona ngati acabe - cabe . 11 : 3 ) Kapena kodi ndi cikondi ca pakati pa mwamuna ndi mkazi ? ( Yesaya 65 : 17 ; 2 Petulo 3 : 13 ) Yehova adzakupatsani madalitso amenewa ngati mukhalabe okhulupilika kwa iye . Ngakhale n’conco , Yesu anaticenjeza kuti tiyenela kupewa maganizo aciwelewele . Iwo ndi atsogoleli akhungu . ” Pofuna kuwononga anthu oipawo , Yehova anabweletsa Cigumula ca Nowa . Iye amafuna kuti mtendele ukhale mbali ya umoyo wawo . Kumbukilani kuti mu mpingo mumapezeka anthu a mitundu yosiyana - siyana amene Yehova wawakokela kwa iye . ( Yoh . Koma Yehova amafuna kuti anthu ake asamangopewa kunama cabe . Mwacitsanzo , m’malo mopeleka mndandanda wa malamulo ambilimbili , Yesu anapeleka lamulo limene limachedwa Khalidwe Lopambana . Ndinali kukonda kuthandiza anthu odwala ndi ovulala , ndipo ndinali kufuna kudzakhala dokotala wa opaleshoni . Baibulo limafotokoza za boma lotelo . Ndiyeno mwayamba kuthaŵila ku nyumba ya mnzanu imene ili pafupi . 7 : 1 ) Ikambanso kuti : “ Izi zimaonetsa kuti munthuyo sacita khama kuti azicita zinthu zoyenela ndi kukhala wodziletsa . Tikadzamasulidwa ku ukapolo wa ucimo , m’pamene tidzakhala na ufulu weni - weni ngati umene makolo athu oyambilila anali nawo . Katswili wina wa zam’nkhalango anakamba mosapita m’mbali kuti : “ Kunena zoona , sitidziŵa kuti tingayambile pati kukonza pulaneti lathuli . ” Yesu anati tiyenela kukonda mnzathu mmene timadzikondela . Ndithudi , Baibulo limatsutsa mgwilizano wa zipembedzo . ( b ) N’cifukwa ciani tingakambe kuti fanizo la Yesu limaonetsa kuti iye ali ndi cidalilo mwa Akristu odzozedwa ? Pa lemba lina m’Baibo , dzina lakuti Esibaala linalembedwa kuti Isi - boseti , kuonetsa kuti mbali yakuti “ baala ” inaloŵedwa m’malo na mau akuti “ boseti . ” ( 2 Sam . Cinalinso monga mlangizi wawo wowatsogolela kwa Mesiya . ( Agal . M’malo moyenda cozupila , titelo kukamba kwake , tifunika kuyenda moongoka potsatila citsogozo cowongoka ca Yehova . Iye anati : “ Inali nthawi yanga yoyamba kugwila nchito yopelekela cakudya , koma tinasangalala . ” Pa umoyo wanu wonse , mudzayesetsa kusonyeza kuti mumayamikila mphatso imene munalandila . M’baleyo amayamikila kwambili cifukwa woyang’anilayo anakambilana naye mokoma mtima ndiponso mwacikondi . N’ciani cimene tingaphunzile kwa m’busa ndi Msulami ngati tifuna kuloŵa m’banja ? Ngati munatula udindo monga mkulu , kapena ngati munatsitsidwa , ‘ mungayesetse kuti mukhalenso woyang’anila . ’ Molimba mtima , loya wathu anatiteteza mwa kugwila mau a Gamaliyeli wa m’zaka 100 zoyambilila . N’cifukwa ciani tiyenela kukonda Mulungu ndi anzathu ? Kodi pali cifukwa ciliconse cokhulupilila kuti mdani wakale ameneyu adzaonongedwa ? ( Agal . 6 : 4 , 5 ) Komabe , kaya tasankha zosangulutsa zotani , tifunika kuziika pamalo ake oyenelela . Ndipo n’zimene zinacitikadi . Mofanana ndi apainiya anthawi zonse , apainiya apadela amafuna olalikila nao . Mwacitsanzo , m’bale wina asanakhale mboni anali ndi cizoloŵezi copenyelela zamalisece . N’cifukwa cake , atumwi ake ayenela anadzifunsa kuti , ‘ Kodi Yehova adzasankha mtsogoleli watsopano ? ’ Conco , Farao analamula kuti ana onse acimuna aciheberi ayenela kuphedwa akabadwa . N’cifukwa ciani m’pake kuti alambili a Yehova ni anthu a dongosolo ? N’nali kumufotokozela nkhawa zanga , mkwiyo , kukhumudwa , na kudziimba mlandu . Ena amakamba kuti mafunso amenewo alibe phindu cifukwa zamoyo zinacita kusandulika kucokela ku zinthu zina . Yehova amadana kwambili na khalidwe la kunyada na kudzikweza . Zimene okhulupilila zakuthambo osiyana - siyana amalosela zokhudza munthu mmodzi zimasiyana . 12 : 13 ) M’mau ena , tingakambe kuti tinalengedwa n’colinga cakuti tizicita cifunilo ca Mulungu . Anthu oipa adzawapha ndi lupanga , ’ watelo Yehova . Tinakwatilana mu 1957 . Muyenela kulemekeza zinthu zimene akazi anu amakonda ndi kuganizila zimene afuna . * ( Luka 3 : 36 , 37 ) Mwina kucokela kwa anthu amenewa kapena akazi awo , Nowa anaphunzila za ciyambi ca umoyo wa anthu , colinga ca Mulungu codzaza dziko lapansi ndi anthu olungama , ndi za kupanduka kwa mu Edeni . Pa nthawiyo , iye anali kudzionela yekha mavuto obwela cifukwa ca kupanduka kumeneko . ( Gen . Tonse tifunika kukumbukila kuti ndife ocimwa . M’BALE wina na mkazi wake ku France anati : “ Ngakhale kuti timakhulupilila Yehova , sindiye kuti basi ana athu nawonso adzakhala okhulupilila . ” Jowana ndi akazi ena okhulupilila anacitila Yesu zimene anakwanitsa Munthu akadziŵa mwamsanga matenda amene adwala , zingapulumutse moyo wake . Mukadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa , ndiye kuti inuyo panokha mwapanga ubwenzi ndi Mulungu . ( Sal . 147 : 13 , 14 ) Wamasalimoyu ayenela kuti analimbikitsidwa ngako pamene anadziŵa kuti Mulungu adzalimbitsa zipata za mzinda wa Yerusalemu kuti ateteze olambila ake . ( 1 Yoh . 4 : 8 ) M’malomwake , pamene tiphunzitsa ena , tiyenela kugogomeza kufunika kokhala pa ubwenzi wolimba na Mulungu . Kumeneku ndi kumvela kocokela pansi pamtima . ” Moyo wangwilo umene Yesu anapeleka unali wokwanila ndendende ndi zimene Adamu anataya . Kalinde ananifunsa kuti , “ N’cifukwa ciani mukucoka pa nthawi yofunika ngati ino ? ” Yehova amamva mapemphelo athu ndipo amatimvetsetsa kuposa munthu wina aliyense . Tikapeza munthu amene agulitsa ng’ombe , tinali kukamba naye za mmene ng’ombezo zinapangidwila modabwitsa . Anthu ena a m’nthawi yakale , Mulungu anawakonda olo kuti anacitapo macimo aakulu m’mbuyomo . Cenjelani ndi cofufumitsa ca Afarisi ndi ca Herode . ” “ N’zovuta kwambili kuti ana acite coyenela ngati sadziŵa kusiyanitsa cabwino na coipa . ” — Brandon . Kucita zimenezo kukanapangitsa kulambila kwao kukhala kovomelezeka kwa Atate wake . — Mateyu 6 : 1 - 6 . MUZISAMALILA BANJA LANU N’cifukwa ciani tiyenela kukhutila ndi zimene tili nazo ? Mkazi wanga anabwela ku nyumba ali wosangalala . M’malomwake , timaloŵa mu mpumulowo mwa kupitiliza kucita zinthu mwacikhulupililo mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu . Mukaona kuti mwakwiya kwambili , pewani kupeleka cilango mpaka mtima wanu utakhala pansi . Ife ndife dongo ndipo inu ndinu Wotiumba . Tonsefe ndife nchito ya manja anu . ” — Yesaya 64 : 8 . ( b ) ‘ moyo wathu wonse ’ ? Mau a Mulungu Baibo , amaonetsa bwino mmene Iye amaonela umbeta . Iye anati : “ Yesu analangiza otsatila ake kuti afunika ‘ kuwelengela zimene angawononge ’ kuti akwanilitse zolinga zawo . Nchito yao si kumasulila zinenelo zikuluzikulu zokha . Nowa sanafune kugwilizana ndi anthu amene sanali kulambila Mulungu . 12 : 1 - 14 . M’malo moika mtima wake wonse pa nchitoyi , iye anayamba upainiya wa nthawi zonse . NCHITO YOLALIKILA PADZIKO LONSE : Cizindikilo cina conenedwelatu coonetsa kuti tili m’nthawi ya mapeto ndi nchito yolalikila . Baibulo limati : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” N’zoonekelatu kuti pamene Paulo analemba mau akuti Kristu ndi “ cipatso coyambilila ” ca anthu amene adzaukitsidwa , anatanthauza kuti pali ena amene adzauka . Yesu anatiphunzitsa ndi kutionetsa kwa amene tiyenela kupemphela . Ngati afuna kuti tikhulupilile kuti alidi na mphamvu yocita zozizwitsa , atitulutsile madzi m’thanthwe lina ili . ’ ” Mwanayo ndiye anafunika ‘ kupelekedwa kwa Yehova . ’ Nanga mavuto ake tingathane nawo bwanji ? Panthawi yovutayi , Yesu sanafunike ‘ kudzikomela mtima . ’ [ 1 ] ( ndime 12 ) Nthawi zina , atumiki a Yehova sakhala na cakudya cokwanila . Kuti mudziŵe cifukwa cake Yehova amalolela kuti zimenezi zicitike , onani nkhani yakuti : “ Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi ” mu Nsanja ya Mlonda ya September 15 , 2014 , pa tsamba 22 . Mu utumiki wake wa zaka pafupi - fupi 30 , iye anathandiza anthu ambili - mbili kukhala ophunzila a Khristu . ( Mac . 14 : 21 ; 2 Akor . ( a ) Ni malangizo anji amene Paulo anapeleka kwa Timoteyo ? Monga tidzaonela m’nkhani yotsatila , cimene cinawathandiza kukhalabe okhulupilika n’cakuti anali kumudziŵa bwino Yehova . KUDZILETSA ni khalidwe locokela kwa Mulungu . ( Ŵelengani Yesaya 55 : 8 , 9 . ) Nanga Satana angapatsidwe bwanji “ malo kuti akhale manda ” ake padziko lapansi ? Mofanana ndi mmene zingakhalile mukapita kudziko lacilendo , mosakaikila inunso mungayamikile kwambili munthu wina atafotokozelani zinthu zina ndi zina za m’Baibulo . Munthu wina dzina lake Isaac wa ku Kenya anati : “ Ndinapemphela kuti ndimvetsetse Baibulo . Iwo amamvela ciitano cimeneci , ndipo naonso amaitana ena kuti amwe madzi amoyo . KODI tingadziŵe bwanji zimene zili m’mitima yathu ? Koma cifukwa cakuti timagwila nchitoyi mogwilizana , timatha kuphunzitsa anthu ambili za Yehova ndi kuwathandiza kuti azim’tamanda ndi kum’lemekeza . Tingaphunzile zambili kwa anthu ochulidwa m’Baibo amene anali mabwenzi eni - eni , koma amene panthawi ina , ubwenzi wawo unali paciopsezo . Kodi mungawathandize bwanji ana anu kukhutila na zimene amaphunzila na kuzikhulupilila ngati mmene Timoteyo anacitila ? Cleiton , kholo la ana acinyamata aŵili ku Brazil anafotokoza kuti , “ Zimenezo zimacititsa kuti phunzilo likhale laumoyo ndi kuti onse atengemo mbali . ” YEHOVA AMATETEZA ANTHU AKE Iye anali ndi mafunso ambili okhudza tsogolo lake , makamaka pamene anatsala pang’ono kufika . Munthu wangwilo ameneyu anafunika kukhala wokhulupilika kwa Yehova , ndi kukhala wofunitsitsa kupeleka moyo wake kuwombola anthu opanda ciyembekezo . Iye anakamba kuti Sauli ndi mwana wake Yonatani anali anthu “ okondeka ndi osangalatsa . ” ( 2 Sam . ( a ) Kodi ena anali kumvela bwanji pokamba nkhani za m’Sukulu ya Ulaliki ? ( Aroma 12 : 1 ) Barry anakamba kuti : “ Acinyamata amafunika kuphunzila kupanga zosankha pa zifukwa zomveka osati cifukwa ca mmene akumvelela . ” N’cifukwa ciani timamvetsetsa zimene Yesaya analemba za iye mwini ? ( Salimo 145 : 18 , 19 ) Mau awa ni olimbikitsa , si conco ? ( Mlal . 11 : 1 ) Ngati tiyesetsa kupeleka moni kwa ena , maka - maka Akhristu anzathu , timawalimbikitsa , ndipo na ise timalimbikitsidwa . Kodi manyuzipepala ndi wailesi zinali kugwilitsidwa nchito motani polalikila uthenga wabwino ? Alan ataganizila mavuto a m’baleyo , akuzindikila zimene angacite kuti amuthandize , ndipo akufunitsitsa kucitapo kanthu . Idzafotokozanso mmene tingaonetsele makhalidwe amenewa mu umoyo wathu wa tsiku na tsiku ndi muulaliki . Mofananamo , mkulu wina wacatsopano dzina lake Alexandre , anati : “ Pamene ndinali wacinyamata , ndinali kulephela kupemphela pagulu . Yesu anati : “ Kapolo sangatumikile ambuye aŵili , ” Mulungu ndi Cuma . — Mat . Anawagwilitsa nchito yaukapolo wa mtundu uliwonse m’munda , ndi ukapolo wa mtundu uliwonse umene anatha kuwagwilitsa nchito mwankhanza . ” — Eks . Yoyamba , timapeza mtendele mwa kuŵelenga Mau ouzilidwa a Mulungu nthawi zonse . Pambuyo pake , iye anaikidwa kukhala Mfumu . Conco , ndinayembekezela mpaka nditakwanitsa zaka 20 . Ngati ndife odzicepetsa , tidzanena kuti ayi . N’nali Kuopa Imfa ( 1 Pet . 1 : 15 ; Aroma 15 : 16 ) . Kuti tikhale bwenzi la Mulungu , tiyenela kumudziŵa bwino . Zimenezo zikutikumbutsa kuti aliyense payekha ayenela kukhala wokhulupilika kwa Mulungu , wokonzeka , ndiponso kukhala maso . Tiyenela kubwelela kwa iye mofulumila , kufunafuna citsogozo cake , ndi kucitsatila ndi mtima wonse . ( Yes . 9 : 23 ) Kukonda nchito yolalikila , kunalimbikitsa Paulo kucita khama pa nchito yopanga ophunzila . Koma mosayembekezeleka , munthu wina amene simum’dziŵa wadzipeleka kuti aphedwe m’malo mwa inu . Mkwati ndi mkwatibwi amapanga malonjezo awo a cikwati pamaso pa Mulungu ndi pa anthu ambili . Ngakhale zinali conco , anthu ocepa a ku Lusitara anadziŵa kuti Paulo ndi Baranaba sanali milungu yao yonama , koma anali anthu enieni amene anawabweletsela uthenga wabwino . Malemba safotokoza njila imene anthu anali kuyatsila moto m’nthawi zakale . Iye sanafune kuti mwana wake wokondedwa Isaki , akwatile mkazi pakati pa anthu a makhalidwe oipa amenewo . Onani mbili ya moyo wao mu Nsanja ya Olonda ya cingelezi ya November 1 , 1979 . Iye anacilitsa odwala , kudyetsa osauka , na kuukitsa akufa . 5 : 39 , 40 ; Luka 6 : 29 ) * Komabe , cinthu canzelu kwambili ni kupewa zinthu zimene zingakope acifwamba . Mwacitsanzo , ndinaphunzila kuti akufa sadziŵa ciliconse . Iwo amakhala ngati ali mtulo tofa nato . ( Aefeso 5 : 20 ) Mwa mau amenewa zikuonekelatu kuti Paulo analimbikitsa ena kupemphela kwa ‘ Mulungu Atate wake , ’ koma m’dzina la Yesu . — Akolose 3 : 17 . Takamba conco cifukwa nthawi zambili wolakwa amazindikila colakwa cake ndi kucitapo kanthu , ndipo pamakhala palibe cifukwa com’cotsela mumpingo . A George anati : “ Pamene Jordan anafika panyumba , ine ndi mkazi wanga mitima inali itatukutila ndi mkwiyo . Koma pamene anali kutifotokozela tinaugwila mtima . Koma bwanji ngati popanda kudzidziŵikitsa ndi kuuza eninyumba cimene tabwelela , tingofikila kuwafunsa kuti : “ Ngati munali ndi mphamvu yothetsa mavuto , kodi mukanathetsa vuto liti ? ” Umoyo wa kuno ni wopepukilapo cakuti timakhala na nthawi yoculuka yotumikila Yehova . Mosakaikila , Yesu ali nao ndipo akudalitsa khama lao . — Mat . Ndipo anali kulalikila uthenga wa ciyembekezo kwa “ osweka mtima . ” Conco , tingam’funse kuti , “ Kodi munganene kuti cinthu cina sicidzakhalaponso ngati cinthuco sicinakhalepo pa nthawi inayake ? ” Ndiponso , tingalephele kuyamikila mwai umene tili nao wokhala m’gulu la abale apadziko lapansi . M’malomwake , tifunika kukhalabe okhulupilika kwa Yehova ndi kutsatila malangizo ake . ( Mac . 24 : 15 ) Pamenepo ndinayamba kukonda Yehova ndi mtima wonse . ( Onani bokosi lakuti : “ Zimene Mulungu Walosela . ” ) Ena anakamba kuti anayesapo kusiya , koma analephela . Ndi ocepa amene analandila ziphunzitso za Yesu ngakhale kuti iye anali Mphunzitsi wamkulu kuposa onse amene anakhalako padziko lapansi . — Yoh . 6 : 66 ; 7 : 45 - 48 . Mu Ufumu wa Mulungu , anthu adzakhala pamtendele . — Yesaya 32 : 18 . Anauza anthu a mumpingo wa ku Korinto kuti : ‘ Pitilizani kudziyesa kuti muone ngati mukali olimba m’cikhulupililo . ’ ( 2 Akor . Yesu anapeleka citsanzo cabwino kwambili ca mmene tingapewele mayeselo . ( 2 Timoteyo 4 : 20 ) Mnzake wina , dzina lake Epafurodito , nayenso anadwala kwambili cakuti anatsala pang’ono kufa . Koma iye angaganize kuti kucita zimenezo si kofunika kwambili poyelekezela ndi kuthila petulo m’galimoto . N’nali kucita manyazi . 22 Ndise Anthu a Yehova 2 : 17 ) Ndiponso amafuna kuti tizimvela malamulo a boma malinga ngati sawombana na malamulo ake . Mwa kupemphela kwa Mulungu ndi kulola mzimu wake woyela kutitsogolela . A History of the Bible . Ngati mwininyumba sanasankhe , m’baleyo amasankha funso ndi kukambilana naye popanda kumucititsa manyazi . Pa cifukwa cimeneci , Mulungu analangiza amene amasamalila nkhani za ciweluzo kuti : “ Muzifunafuna , kufufuza ndi kufunsitsa za nkhani imeneyo . ” Mitengo ya zinthu zofunika inakwela kwambili cakuti munthu anali kufunika kukhala ndi mamiliyoni kapena mabiliyoni kuti agule zofunikazo . Yehova anapeleka lonjezo lolimbikitsa lakuti : “ Anthu ofatsa adzalandila dziko lapansi , ndipo adzasangalala ndi mtendele woculuka . ” Iye anali kuganizila za mmene Yehova anamuthandizila m’mbuyomo , ndiponso anali kuyembekezela mwacidwi nthawi imene Mulungu adzamupulumutsa . Kuuka kwa Yesu kumaonetsa bwanji kuti Mulungu ali ndi mphamvu ? Motelo , m’malo mokhala ndi malo ena ake apadela , kulambila kwathu kumakhala kovomelezeka kwa Mulungu ngati kumagwilizana ndi zimene Baibulo limaphunzitsa , ndiponso ngati kumatsogoleledwa ndi mzimu woyela . Panthawi ina , ofesi ya nthambi inakonza zoti alongo aŵili ngakhale kuti sanali kumvetsa Cituvalu , aziloŵetsa mau onse pa kompyuta . 32 : 3 , 4 . Mofanana na Davide , anthu a Yehova lelolino amayesetsa kukhala odzicepetsa . Ndikaona zonsezi , ndimadziŵa kuti Yehova amatikonda kwambili . ” ( 1 Tim . 5 : 3 - 16 ) Mofananamo , Yakobo anauzilidwa kulemba za udindo wa Mkristu wosamalila ana ndi akazi amasiye ndi ena amene ali m’mavuto kapena osoŵa . ( Yak . Nanga zingamukhudze bwanji ? ’ “ Anamwali anzake ” a mkwatibwi anadzipeleka kwa Yehova ndipo asonyeza kuti ndi okhulupilika kwa Mfumu yao . Yesu anauza otsatila ake kuti ayenela ‘ kukhalabe maso . ’ ( Mat . Iwo ayenela kupeza nthawi yotsimikizilana kuti amakondana mwa mau ndi zocita zao . Nkhani ya m’Baibulo ya Akani ionetsa mmene umbombo ungakhalile wamphamvu . Rutherford woimila likulu lathu anacititsa msonkhano m’dela limenelo ndipo kunapezeka anthu 2,000 . Anthu ena amaganiza kuti Mulungu saona zimene io amacita . 19 : 5 , 15 - 20 ) Cinanso , Hezekiya anaonetsa nzelu mwa kupeleka ndalama zimene Senakeribu anam’lamula kuti apeleke . ( 2 Maf . Anapemphanso kuti amucilitse . Kodi colinga ca moyo n’ciani ? Anawadzoza na mzimu woyela ndi kuwapatsa mwayi wokhala ana ake auzimu . 102 : 20 , 21 . Popeza kuti palibe munthu amene angacite zimenezi , n’zoonekelatu kuti lembali likamba za Mlengi wathu . Koma sanali “ kuopa anthu . ” ( Miy . Mwacitsanzo , Yehosafati anacita mgwilizano wacikwati ndi Ahabu , Mfumu yoipa ya ufumu wa kumpoto wa Isiraeli . Posacedwapa , Jumpei na Nao nawonso analoŵa Sukulu ya Alengezi a Ufumu . Masiku otsiliza ano , makhalidwe a anthu afika poipa kwambili . Kwa zaka zambili , tinali kukhulupilila kuti anthu anali kuweluzidwa kupyolela m’nchito yolalikila imene ikucitika m’nthawi ino ya mapeto . Ngati munthu walandila uthenga wathu , anali kuweluzidwa kuti ndi nkhosa , ndipo ngati wakana , anali kuweluzidwa kuti ndi mbuzi . 5 : 4 ) Mwana wawo woyamba , Kaini , anakwatila mkazi wa m’banja mwawo . Koma motsogoleledwa na Yehova , masiku ano tikucita zambili kuposa kale lonse . Kunalibe mankhwala ocilitsa khate pa nthawiyo . 4 : 13 ) Cifukwa Yehova Mulungu ndi wacikondi , amalakalaka kuukitsa akufa , makamaka anthu okhulupilika ndi olungama monga Yobu . Kodi ndikanacita zinthu mwanzelu ? ’ Mwacikondi , Yehova anatipatsa malamulo na mfundo zimene zingatithandize kuphunzitsa bwino cikumbumtima cathu na kuona zinthu mmene iye amazionela . “ Kukonda ndalama ” kungacititse munthu . . . Tumikilani Yehova Popanda Cosokoneza Koma iye anaukana uphungu wawo . 45 : 13 ) Kodi “ mfumu ” imeneyi ndani ? Mu 1931 , ku Mexico kunali ofalitsa 82 . Ni kusaganiza bwino kuleka kuika zinthu za Ufumu patsogolo cifukwa cofuna cabe kupeza zinthu zambili zakuthupi . Kodi kuthaŵila kwa Yehova kutanthauza ciani ? Iye amangotiuza kuti monga Akhristu , tifunika kuvala na kudzikongoletsa moyenelela . ( 1 Tim . 2 : 9,10 ) Mulungu amafunanso kuti tizipewa zosankha zimene zingakhumudwitse kapena kusokoneza ena . ( 1 Akor . Wolemba Baibulo Yuda analemba za kudzicepetsa kwa Yesu asanabwele padziko lapansi . N’ciani cidzacitikila anthu oipa ? — Vesi 10 . Kodi zinthu zasintha bwanji masiku ano ? Ciŵelengelo cimeneci cimaposa ziŵelengelo zonse za m’mbuyomu . Nthawi zina , nafenso timafuna kudziŵa nthawi pamene malonjezo a Mulungu adzakwanilitsidwa . Pambuyo potsatila malangizowo , mukuona kuti mwayamba kugona bwino tsopano . Ndipo kucita zimenezo n’kofunika cifukwa ndi mmene moyo wanu udzakhalile kudzikolo . Mtumwi Paulo anakamba kuti Akristu akhoza ‘ kulimbikitsana mwa cikhulupililo . ’ Kodi mwakhala pa ulova kwa nthawi yaitali ngakhale kuti mumayesetsa kusakila nchito ? Paulo anali mlembi wa Baibulo woyamba kugwilitsila nchito fanizo limeneli . Mungacite ciani kuti muzikhala wokhulupilika kwa Yehova ndi Ufumu wake ? Zimene Nowa sakanakwanitsa kucita : Olo kuti Nowa analalikila za cenjezo la Yehova mokhulupilika , iye sakanatha kuumiliza anthu oipa kulandila uthengawo . Sakanathanso kufulumizitsa Cigumula . Nthawi yonseyi , mkazi wanga anali ndi nkhawa cifukwa sanali kudziŵa kumene ndinali . Acicepele ena kumeneko anamupempha kuti aloŵe kilabu yawo ya maseŵela . Ndipo anthu olembedwa m’Baibulo amene anaukitsidwa ndi ocepa poyelekezela ndi anthu amene Mulungu akulakalaka kudzaukitsa . Nthawi zonse , mdzukulu wao wamwamuna wa zaka 6 anali kuwasungila malo okhala , ndipo ngati a David sanabwele kumisonkhano , mdzukuluyo anali kuwauza kuti , “ Ndinakusoŵani kumisonkhano lelo Ambuya . ” Ayuda ambili naonso anayamba kukamba Cigiriki , kenako Malemba Aciheberi anamasulidwa m’Cigiriki . Nthawi ina Petulo anafunsa Yesu ngati tifunika kukhululukila ena “ mpaka nthawi 7 . ” Yesu anamuyankha kuti “ Ndikukuuza kuti , osati nthawi 7 zokha ayi , koma , mpaka nthawi 77 . ” Zoonadi , Yehova wanidalitsa ngako . — Sal . Nkhani izi zidzatithandiza kuyamikila kwambili cikondi cacikulu cimene Mulungu amationetsa mwa kutipatsa cilango monga Tate wathu . Koma kodi abale na alongo amenewa anacita ciani kuti akwanitse kukukila ku Myanmar ? Baibulo limatiuza kuti : “ Musamatengele nzelu za nthawi ino . ” NYIMBO : 126 , 150 Limatanthauza “ Mfumukazi . ” Kodi Zidzatheka Kukhala M’dziko Lopanda Nkhanza ? Ana anu akakula zidzawathandiza kusankha amene adzatumikila . Atabeleka mwana wamwamunayo , iye anati : “ Ndinam’pempha kwa Yehova . ” — 1 Sam . Madalitso a Yehova anacita kuonekelatu cakuti lomba m’delali muli mipingo yambili . Ngati mungadziŵe pasadakhale kuti kudzabwela cimphepo coononga mungacitepo kanthu kuti mudzapulumuke . Pamene alalikila uthenga wa Ufumu , ofalitsa acatsopano afunika kudziŵa kuti kuleza mtima n’kofunika . Ndiyeno , tingawafotokozele kuti tifuna akasangalale pa cikwati cao . M’nthawi ya Atumwi , anthu masauzande ambili anali kupita ku Yerusalemu kukacita zikondwelelo zimenezi . Zimene takambazo zionetsa mtundu wa zilembo zimene Hutter anaseŵenzetsa m’Baibo yake ya Ciheberi pa Ezekieli 18 : 4 , zimene zipezekanso m’mau amunsi mu Reference Bible pa vesi imodzi - modziyo . Tengelani citsanzo ca Yesu mwa kuwathandiza kuti azisangalala pophunzitsa ena Mau a Mulungu . Koma Nabala , amene dzina lake limatanthauza “ Wopanda nzelu , ” kapena “ Wopusa , ” anacita zinthu mogwilizana ndi dzina lake . 3 : 7 ) Amuna angaonetse kuti amaona akazi ao kukhala a mtengo wapatali mwa kulankhula nao mwaulemu ndi mokoma mtima kaya ali pamaso pa anthu kapena ali paokha . ( Miy . Izi zinapangitsa kuti pacitike zinthu zimene sitinali kuyembekezela . 4 : 17 ) Komabe , ana asanabatizike , makolo amafuna kutsimikizila kuti anawo ni okonzeka kukwanilitsa udindo wokhala wophunzila wa Khristu . Ndiyeno akulu anakonza zakuti woyang’anila dela akamuyendele . ( Miy . Conco kukabwela alendo , tiyenela kuwalandila , mosasamala kanthu za maonekedwe kapena kavalidwe kawo . ( Yak . N’ciani cinacititsa kuti Petulo kuazindikile kuti Yehova alibe tsankho ? Onani mmene a George ndi a Nicole , makolo aŵili amene tachula kuciyambi kwa nkhani ino , analangila ana ao . Mu 1964 , Arthur analandila utumiki watsopano , wokhala mtumiki wa nthambi ku Irish Republic . Ni njila zina ziti zimene anthu a m’cikwati angaonetsele kuti amacilikiza ulamulilo wa Yehova ? Mtumwi Paulo ananena kuti ngati Akristu acikulile sangathe kudzipezela zofunikila , ana ndi adzukulu ayenela ‘ kubwezela makolo ndi agogo ao zowayenelela . ’ Yesu anakamba kuti : “ Conco ngati wabweletsa mphatso yako paguwa lansembe , ndipo uli pomwepo wakumbukila kuti m’bale wako ali nawe cifukwa , siya mphatso yako patsogolo pa guwa lansembe pomwepo . Pocita ulaliki umenewu , mlongo wina anapatsa adilesi ya imelo yake kwa mtsikana wina amene analandila bukuli . Pamene Abulahamu anadziŵa koyamba kuti Yehova adzadalitsa Sara mwa kum’patsa mwana , “ anagwada n’kuŵelama mpaka nkhope yake pansi , n’kuyamba kuseka . ” Panali nthawi zina pamene Davide anavutika kwambili . “ Kuimbila Mulungu wathu nyimbo zomutamanda n’kwabwino . ” — SAL . * Ndiye cifukwa cake iye anatipatsa Mau ake , si conco kodi ? Lana anafika kwao bwinobwino ndipo anapitiliza kutumikila monga mpainiya wa nthawi zonse . Wamasalimo Davide anadziŵa kuti Yehova ndiye “ kasupe wa moyo . ” ( Akolose 4 : 6 ) Nthawi zonse tikamafotokoza zimene timakhulupilila , timacita zimenezi “ ndi mtima wofatsa ndiponso mwaulemu kwambili ” cifukwa timakonda anzathu — 1 Petulo 3 : 15 . Iye sacita zinthu monga Bilimankhwe amene amasinthasintha maonekedwe ake malinga ndi malo . ( Luka 22 : 43 ) Yesu anali ndi cidalilo cakuti Yehova adzatumiza angelo kudzamuthandiza akafuna thandizo , kuti akwanilitse cifunilo ca Mulungu . — Mat . Timalephela kukhulupilila ngati amene wamwalila ndi wokondedwa wathu . Anthu okwatilana angalimbitse cikwati cao ngati amaganizila mmene mnzao wa mu cikwati akumvelela . Yosefe anakamba kuti Farao adzabwezela wopelekela cikhoyo pa udindo wake wakale . Iwo anakhalabe okhulupilika kwa Yehova ndi kwa wina ndi mnzake . Ndiye cifukwa cake ifenso tiyenela kukhululukila ena . N’cifukwa ciani n’zotheka kukonda Yehova ? M’nkhani yapita , tinaphunzila cifukwa cake kudzicepetsa kukali kofunika masiku ano , na mmene tingakuonetsele . Motelo , nthawi zonse tiyenela kucita cifunilo ca Yehova ngakhale pamene sizitikomela . Zimenezi n’zosadabwitsa cifukwa cakuti mwacibadwa mwana aliyense amatengela atate ndi amai ake . Munthu wacifundo amayesetsa kuthandiza anthu amene akuvutika , mwina mwa kuwathandiza kuthetsa vuto lawo . Koma amaphunzila citundu canu maka - maka ngati mukamba nawo kaŵili - kaŵili m’citundu canuco . Iwo akaphunzila citundu canu , zimathandiza kuti muzikamba nawo momasuka . Koma palinso mapindu ena . 2 : 3 , 4 ) Nanga tingacite bwanji zimenezi ? N’ciani cinacititsa Baibo ya King James Version kukhala yochuka ? Masiku ano , Riana akupitiliza kulalikila uthenga wa Ufumu kwa anthu ambili okamba Citandiroyi , amene afuna kuphunzila za Yehova . Koma mau akuti “ inu ” ndi akuti “ anthu inu , ” akusonyeza kuti likukamba za anthu ambili osati munthu mmodzi . Iye amatitsimikizila kuti tidzalandila madalitso ngati tipeleka cuma cathu pocilikiza Ufumu wake . ( Mal . N’cifukwa ciani tiyenela kuyesetsa kuona zabwino mwa ena ? Iwo analimbikitsa ine , pamodzi na mwana wawo wamkazi wamng’ono Nora , kuti tiyambe upainiya . Kumbukilani kuti akulu amatikonda ndipo amafuna kuti tikule mwauzimu . Kuonjezela apo , abambo ake a John anadwala matenda aakulu ndipo anafunika cisamalilo ca banja . N’zokondweletsa cotani nanga kuona mmene abale na alongo akuseŵenzetsela mwanzelu ufulu wawo potumikila Yehova ! — Sal . Kodi malangizo apa 1 Timoteyo 4 : 8 ndi Miyambo 13 : 20 angatithandize bwanji posankha zosangulutsa ? Komanso , iye anawafotokozela fanizo la mtengo wa mpesa , limene tinakambilana m’nkhani yapita . 34 : 14 . Nkhanizo zinathandizila kufalitsa uthenga wabwino , ndipo mipingo inabadwa m’mizinda yambili m’dziko lonse la Ireland . — Za m’nkhokwe yathu ku Britain . Komabe , pakangopita miyezi ingapo , iwo angafunike kumadzisamalila okha . Conco anawafunsa kuti : “ N’cifukwa ciani nkhope zanu zili zacisoni lelo ? ” Nkhani yoyamba imene tinakambilana ndi ya Utatu , ndipo anandiuza kuti si ciphunzitso ca m’Baibulo . Khalidwe la kukoma mtima tidzalikambilana m’tsogolo , m’nkhani ina yofotokoza cipatso ca mzimu . Yesu anakamba kuti ngati ticita zimenezi “ [ zinthu ] zina zonsezi zidzawonjezedwa ” kwa ife . Kuphika mkate ndiye inali nchito yotsatila ya tsiku ndi tsiku . Anthu ambili amacita cidwi akadziŵa kuti dzina la Mulungu limachulidwa nthawi zambilimbili m’mipukutu yakale Maulendo aubusa amene akulu amacita amatipatsa mwayi wopeza nzelu zocokela m’Mau a Mulungu ( Onani palagilafu 18 , 19 ) Koma zimene ndikuuza inuzi ndikuuza onse , Khalani maso . ” — Maliko 13 : 33 - 37 . Tsopano mmelawo utakula ndi kutulutsa ngala , namsongole nayenso anaonekela . ” Nanga zimenezi zimatanthauzanji kwa Akristu ? Kodi atsogoleli a cipembedzo anacita ciani ndi Wycliffe , Baibo yake , ndi otsatila ake ? Akatswili oona pa zaumoyo wa anthu , apeza kuti anthu mamililiyoni amaona kuti kupemphela n’kofunika . Mukacita conco , ndiye kuti Mfumu yathu amenenso ni Mkulu wa Ansembe , kuphatikizapo okwela pa mahosi akumwamba , adzapitiliza kukutetezani . M’NTHAWI ya Akhristu oyambilila , anthu a mu Ufumu wa Roma anali kunyadila kuti anali odziŵa bwino za malamulo na cilungamo , ndiponso kuti anali na ufulu . Iye anathandizidwa ndi mnzake Antonio , panthawi imene zinthu zinali zovuta pa umoyo wake . N’cifukwa cake timasangalala na ukulu wa cilengedwe , zodabwitsa za m’cilengedwe , mapikica okopewa mwaluso , nyimbo , komanso ndakatulo . Ndipo sindifuna kuti ndidzaononge ubwenzi wanga ndi mwana wanga . ” Mwana wake Yesu anati : “ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi maganizo ako onse . ” Ndiyeno dzifunseni kuti : Nthawi zina , iye anali kumvela malamulo a Mulungu . ( Yos . 20 : 4 ) Pakapita nthawi , wolakwayo anali kum’tumiza kwa akulu a mumzinda umene anaphela munthu , ndipo akulu a kumeneko ndiwo anali kuweluza mlandu wake . 17 N’cifukwa Ciani Tifunika Kutamanda Yehova ? Nanga n’cifukwa ciani imwe muyenela kukhulupilila kuti mtsogolo akufa adzauka , kuphatikizapo okondedwa anu ? Ngati munthu alephela kuyembekezela kapena kuleza mtima , koma acita zinthu zimene alibe nazo cilolezo , kumeneko ndiye kudzikuza , kapena kuti kudzimvela . 15 : 20 ; 2 Sam . KODI Mulungu amafuna kuti Akristu oona azipita ku nkhondo kukapha anthu amitundu ina ? Pambuyo pa ubatizo , ophunzila onse afunika kupitiliza kukula m’cidziŵitso colongosoka . Lemba la Chivumbulutso 21 : 14 , limanena za maziko okwanila 12 , amene anali ndi maina a atumwi 12 . Kodi n’zocitika ziti zimene zingatiike paciyeso pa nkhani ya kudzicepetsa ? 3 “ Inali Mphatso Yabwino Koposa Imene Sin’nalandilepo ” ( Onani ndime 13 ndi 14 ) Pofuna kuti Baibulo lipezeke m’zinenelo zinanso , omasulila mabuku akhala akugwila nchito mwakhama . Iwo amakumbukila kuti kale mipingo inali kutsogoleledwa ndi mtumiki wa mpingo m’malo mwa bungwe la akulu , nthambi ya m’dziko lililonse inali kuyang’anilidwa ndi mtumiki wa nthambi m’malo mwa komiti ya nthambi , ndipo malangizo anali kupelekedwa ndi pulezidenti wa Watch Tower Society m’malo mwa Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova . Kodi zioneka kuti n’cifukwa ciani Mulungu sanavumbule zambili zokhudza Satana , Mesiya asanabwele ? 2 : 25 . 19 : 13 ) Kodi “ kucita modzikuza ” kumatanthauza ciani ? Koma cimene tikudziŵa n’cakuti Yaeli anacitapo kanthu mwamsanga , ndipo Sisera anaphedwa . — Oweruza 4 : 18 - 21 ; 5 : 24 - 27 . Kodi imeneyi ni nkhani yomvetsa cisoni ? N’cifukwa cake Yesu popemphela kwa Atate wake anati : “ Mau anu ndiwo coonadi . ” Colinga cathu ndi kukhalabe wokhulupilika kwa Mulungu . N’takwanitsa zaka zitatu mu upainiya , m’bale Earl Stewart wocokela ku ofesi ya nthambi , anakamba nkhani pa msonkhano wa anthu oposa 500 , umene unacitikila pa bwalo lina m’tauni ya Angat . Linali tsiku limene n’nabatizika pa msonkhano wacigawo wa Mboni za Yehova . Kuti ana aphunzile makhalidwe abwino , kuphatikizapo khalidwe la kudziletsa , makolo mufunika kupeleka citsanzo cabwino . Ana anu adzapindula kwambili ngati aona kuti nthawi zonse inu mumalalikila , kupezeka pa misonkhano , ndi kucititsa kulambila kwa pabanja . Nafenso tingacite zinthu zina - zake zabwino kwambili , ndipo Yehova ‘ angatisiye kuti atiyese ’ ndi kuona zonse zimene zili mumtima mwathu . Cifukwa ca kumenyedwa kwa kale - kale , nthawi zina miyendo ndi thupi lonse zimaŵaŵa , maka - maka nikacoka muulaliki . Ena a inu mwakhala mukusangalala ndi madalitso amenewo kwa zaka zambili , ndipo malinga ndi zimene taona tikuvomeleza kuti palibe njila ina yamoyo imene ingabweletse cimwemwe . — Sal . Mudzapindulanso ngati musinkhasinkha musanapite mu utumiki . Ambili a ise tingavomeleze kuti zoŵelenga - ŵelenga sitizikonda komanso kuphunzila kumativuta . 5 , 6 . ( a ) Ni makonzedwe ati amene anapangidwa m’dziko lina pofuna kulimbitsa mgwilizano pakati pa anthu a Mulungu ? ( Agalatiya 5 : 22 , 23 ) Iye amaonetsanso kufatsa , kudziletsa ndiponso kuleza mtima . Ngakhale kuti mungakwatiwe kwa munthu wokoma mtima amene satumikila Yehova , kodi ubwenzi wanu ndi Yehova ungakhudzidwe bwanji ? Fanizo la Yesu litiphunzitsa kuti tiyenela kukonda anzathu ndi kuwacitila cifundo . ( Luka 5 : ​ 34 , 35 ) Nanga bwanji za anamwali ? Anapitiliza kucilikiza mwamuna wake paulendo wawo wokuka - kuka , kum’thandiza kulonga matenti , kutsogolela ziŵeto , na kumanga misasa . Iwo atumikila ku malo kumene kufunika olengeza Ufumu ambili . Nayenso Louis anati : “ Tangoganizilani ! Pa Cikumbutso cimene tinacita nawo koyamba m’dziko la Madagascar , maphunzilo athu a Baibo 10 anapezekapo . ” “ INE ndi makolo anga tinasamukila m’dziko lina , ndipo pamene n’nali mwana n’nali kukamba citundu cawo kunyumba na kumisonkhano , ” anatelo Joshua . Masomphenya a namba 8 , adzatithandiza kuona mmene Yehova amatetezela olambila ake kuti kulambila koona kupitilize . Iye amatilonjeza kuti imfa idzagonjetsedwa . Koma sindikumbukila kuti ndinaonako paliponse pamene panalembedwa caka ca 1914 . 2 : 41 ) Pambuyo pake , atumwi anapitiliza kugwila nchito yolalikila mwakhama ndi kubala zipatso . ( Mac . Nanga zimenezi zikutikhudza bwanji ife amene tikukhala pa “ copondapo mapazi ” ca Mulungu ? Pambuyo pakuti motoka yawo yawonongeka , M’bale Keltie , amene anali na mwendo wopanga , anapitiliza ulendo wolalikila umenewo poseŵenzetsa ngamila . ( Mateyu 7 : 12 ) Mukalakwa , olo kuti colakwaco n’cacing’ono , mumafuna kuti anthu akucitileni zinthu mwacikondi kapena kunyalanyaza colakwaco . Mwacitsanzo , ngati munthu angafunse funso limodzi - modzi lokhudza zam’tsogolo kwa anthu aŵili “ oseŵenzetsa ” makhadi a njuga za matsenga , mwacionekele mayankho awo afunika kufanana . Akristu acikulile sayenela kuona kuti nkhani zimene amalembela acinyamata n’zosafunika kwa io . Atamaliza kuloŵetsa nyama m’cingalawa , “ Yehova anatseka citseko . ” — Gen . Malinga ndi 2 Akorinto 4 : 16 , 17 , tatsimikiza mtima kucitanji ? Mwina Yesu anali kuganizila za “ maluwa ” okongola osiyanasiyana . Conco , tingam’funse kuti , “ Ngati Adamu ndi Hava anayenela kulandila cilango camuyaya atacimwa , kodi sizikanakhala bwino kuwacenjezelatu ? ” Nthawi imeneyo , zaka zoposa 5,000 zapita , anthu anali kukhala na moyo zaka zambili kuposa masiku ano . 4 / 1 Cifukwa sanaiŵale mmene iye analili poyamba . Yehova sananyalanyaze bodza limeneli . Pali cifukwa cacitatu cimene cimatipangitsa kukhulupilila kuti mapeto ali pafupi . Uthenga Wabwino wa Mateyu , Maliko , Luka , na Yohane Koma ngati timayesetsa kugwila nchito yathu mwakhama , ngakhale ioneke yosasangalatsa kapena yovuta , timakhala osangalala cifukwa codziŵa kuti tacita zamphamvu . Munthu aliyense angayambe kuonetsa mzimu wodzikweza ngati agonja ku zilakolako za thupi . ( Machitidwe 17 : 24 , 25 , 28 ) Yehova amatipatsa zinthu zonse zimene timafunikila kuti tikhale moyo ndi kusangalala . Iye anati : “ Kuleka kuyenda si kutha kwa ulaliki wanga . Ena amaika tuakacisi m’nyumba zao . Anadziŵa kuti ngati apitiliza kucilikiza zipembedzo zonama , sangalandile madalitso a Mulungu . Ndinakwanitsa kusamalila banja langa mwakuthupi ndi mwa kuuzimu cifukwa ca thandizo la Lidasi mkazi wanga . Conco , ndinapita ku sukulu ina ya ku Bad Hofgastein , tauni ya m’mbali mwa mapili a Alps . ( b ) Ndi khalidwe liti limene limagwilizana ndi lemba la Aefeso 4 : 25 ? Iwo anali kulalikila za uthenga wabwino umene m’Yuda aliyense wokhulupilika anali kufuna kuumva . Uthengawo unali kunena za kubwela kwa Mesiya ndi kukwanilitsidwa kwa maulosi okamba za iye olembedwa m’Malemba . Pambuyo pake , padziko lonse padzakhala mtendele woculuka . Anawauza kuti azipemphela kuti : “ Mutipatse ife lelo cakudya cathu calelo . ” ( Mat . N’zomvetsa cisoni kuti mu 2015 amuna anga anamwalila na khansa ya mu ubongo . 6 : 2 ; 19 : 11 ) Kuonjezela pa lupanga , mfumu yanyamulanso uta . 2 : 14 , 15 . Iye sawakakamiza kusintha , koma amawaphunzitsa miyezo yake yolungama . Tikutelo cifukwa mudzatha kudziŵa zimene anawo amakamba , zosangulutsa zimene amakonda , ndi zimene amaphunzila kusukulu . Mudzathanso kukambilana mosavuta ndi matica awo . 15 , 16 . ( a ) Kuti tikhale monga Khristu , kodi tifunika kucita ciani ? Mfundo zimenezi na zina ndiye zinacititsa Mulungu kupatsa anthu mphatso yopambana zonse . Sinikayikila kuti ni cifunilo ca Yehova kuti nizitumikila kuno ku Mandalay . ” N’cifukwa ciani Akhristu safunika kuona cikwati mopepuka monga mmene anthu a m’dzikoli amacitila ? ( Chiv . 7 : 14 ) Kodi timagwilizana ndi anthu onse , kuphatikizapo aja amene timaona kuti ndi a mtima wapacala ? Mau a mtumwi Petulo angatithandize pankhaniyi . Lemba la 1 Timoteyo 3 : 1 limati , “ ngati munthu aliyense akuyesetsa [ kapena kuti kukalamila ] kuti akhale woyang’anila , akufuna nchito yabwino . ” Tingaonetse bwanji kuti timaona moyo mmene Yehova amauonela ? Cimene cingatithandize kukhala na cikhulupililo colimba si kuŵelenga Baibo cabe . 34 : 9 ) “ Gidiyoni anagwidwa ndi mzimu wa Yehova . ” Ndiyeno anasuliza zimene Baibo imakamba pankhani ya ciwelewele , ndipo ananikakamiza kuti tiyambenso cibwenzi . Cifukwa cakuti adzakuthandizani kuona kuti ubatizo ndi nkhani yaikulu . Makolo acikhiristu amaonetsa kukhulupilika kwawo kwa Yehova mwa kuphunzitsa ana awo mogwilizana na Mau a Mulungu . Kodi io anacita ciani pamene zinthu zina zimene anali kuyembekezela sizinacitike m’caka ca 1914 ? Koma mwina mungadzifunse kuti , ‘ Kodi mgwilizano weni - weni ungakhalepo bwanji ? ’ Kucokela mu 1919 , Yehova anayambanso kusonkhanitsa odzozedwa . Amenewa ndiwo akuimilidwa na ndodo “ ya Yuda . ” ( Genesis 18 : 6 ) Ena anali kuphikila mikate yao pa miyala yothentha ; ena anali kugwilitsila nchito tumauvuni tung’onotung’ono . Zitadziŵika kuti umboniwo unali wabodza , maloya anacita khama , ndipo mmodzi wa oimbidwa mlanduwo anamasulidwa . Amuna okhwima mwa kuuzimu amenewa angakhale “ malo obisalilapo mphepo ndi malo ousapo mvula yamkuntho , ngati mitsinje yamadzi m’dziko lopanda madzi , ndiponso ngati mthunzi wa thanthwe lalikulu m’dziko louma . ” ( Yes . N’zoona kuti aliyense wa ise afunika ‘ kupitiliza kukonza cipulumutso cake , mwamantha ndi kunjenjemela . ’ ( Afil . Iye anali wanzelu ndi wodziŵa bwino Malemba ndipo anali citsanzo cabwino kwa tonse . M’bale Franz anali kutikonda tonsefe . N’cenjezo liti limene Yohane anapeleka la mmene tiyenela kukondela Mulungu ? ( Luka 6 : 31 ) Apa Yesu anatanthauza kuti tiyenela kucitila ena zinthu zimene tifuna kuti io aticitile , ndi kupewa kubwezela coipa pa coipa . Posakhalitsa , Kazuhiro analembela imelo ofesi ya nthambi ya ku Myanmar na kufotokoza kuti iye na mkazi wake akulakalaka kukatumikila m’dzikolo monga apainiya . Ena amafika poona nchito yolalikila monga mankhwala . 5 , 6 . ( a ) N’ciani cimene Yesu anacita cifukwa cokonda ophunzila ake ? Wadela wina analemba kuti : “ Pamene n’nali wacicepele , n’nali na mafunso ambili mu mtima mwanga . Mwacitsanzo , ganizilani mmene mneneli Natani anamvelela pamene anapita kukakamba na Mfumu Davide za chimo lake lalikulu limene anayesa kulibisa . Baibo imafotokoza cifukwa cake . Mwacitsanzo , Baibulo limati : “ ‘ [ Mulungu ] adzapukuta misozi yonse m’maso mwao , ndipo imfa sidzakhalaponso . Antonio , amene atate wake anamwalila pangozi ya galimoto , anati : “ Zimakhala ngati winawake wakhoma zitseko zonse za nyumba yanu ndi kutenga makiyi ndipo sungakwanitse kuloŵa m’nyumba . Poyamba , io anali kuona kuti sanali kucita zambili mu utumiki . Ngakhale kuti tatumikila Yehova kwa nthawi yaitali kapena ai , aliyense wa ife ayenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi pali zinthu zina zimene ndingasinthe kuti nditsatile Yesu mosamala kwambili ? N’cifukwa ciani tinavomeleza utumikiwo ? Anthu othaŵa kwawo angakumane ndi mavuto pamene athaŵa kapena pamene akhala m’kampu ya anthu othawa kwawo . Komanso tinali kupezeka pa misonkhano yonse ya Mboni za Yehova ku Nyumba ya Ufumu . CIYEMBEKEZO CA M’BAIBULO Conco , ngakhale wacicepele angathe kusiyanitsa cabwino ndi coipa ndiponso angathe kudzipeleka kwa Mlengi wake . Kodi zinacitika bwanji kuti akulu - akulu a chechi akhale na mphamvu zonse pa Baibo ? M’nkhani imeneyo , muli malemba aŵili amene angakuthandizeni pofotokozela ena zikhulupililo zanu . Iwo anandithandiza kuti ndizikhulupilila kwambili Mulungu . Nthawi zambili anthu m’dzikoli amayamikila Mboni za Yehova cifukwa cakuti ndi anthu oona mtima . Mosiyana ndi kanjele ka mpilu kamene kukula kwake kumaonekela mosavuta , kufalikila kwa zofufumitsa sikuonekela nthawi yomweyo . Kumbukilani zimene zinacitika pamene Paulo na Baranaba anali ku Antiokeya wa ku Pisidiya . N’cifukwa ciani nimakhulupilila kuti kutsatila mfundo za m’Baibo n’kopindulitsa pa umoyo wanga ? ’ — Yes . M’mwezi wa Nisani m’caka ca 1513 B.C.E . , Yehova anatuma Mose ndi Aroni kukapeleka malangizo awa kwa Aisiraeli : Sankhani nkhosa yaimuna kapena mbuzi yopanda cilema , muiphe ndi kuwaza magazi ake pamakomo a nyumba zanu . ( Eks . Kodi dipo limapindulitsa bwanji ( a ) Akristu odzozedwa ? Koma pamafunika khama kuti mupitilize kukhala pa ubwenzi na Mulungu na kukonza cipulumutso canu . Inshuwalansi : Mungakonze zoti gulu la Yehova lidzalandile ndalama za inshuwalansi kapena za penshoni . Kuyambila m’buku la Genesis mpaka Chivumbulutso , Baibulo lili ndi zitsanzo zoonetsa kuti Yehova nthawi zonse amagaŵila nchito ana ake auzimu . Zimene timacita pa malonjezo amene tinapanga zimakhudza ubale wathu na Yehova . Yehova anam’dalitsa kwambili Mariya cifukwa com’tumikila mokhulupilika . Yesu wagwilizanitsanso anthu okhulupilika oposa 7 miliyoni , ndipo onse adzipeleka kucita cifunilo ca Atate wake . ( Sal . Sitiyenela kuleka kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova . Mu 1524 , atatsiliza kumasulila Malemba a Cigiriki ( ochedwa Cipangano Catsopano ) , anafalitsa buku la Masalimo la m’Cifulenchi n’colinga cakuti Akhiristu azipemphela “ modzipeleka kwambili ndi mokhudzika mtima . ” Kuvomela kuphunzila Baibulo kapena kuleledwa m’coonadi pakokha sikupangitsa munthu kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova . Ndiye cifukwa cake anacita pangano na maso ake kuti asayang’ane namwali mom’khumbila . Acinyamata a Mboni amenewo sacita mantha kuti adzakakamizidwa kucita zinthu zimene zingasokoneze ubwenzi wao ndi Yehova . Ndiyeno m’nkhani yotsatila , tidzakambilana za kulimba mtima ndi kuzindikila . Zonse zimene zakhala zikucitika pa kulambila koona masiku otsiliza ano , ni umboni wamphamvu wakuti Yehova akutidalitsa ndi kuti Khristu akutitsogolela . Monga takambila kale , mtima wonyada unacititsa kuti atumwi ake asakhale ogwilizana kweni - kweni . ( a ) N’cifukwa ciani kulimbana ndi Satana n’kofunika kwambili masiku ano ? Pofuna kuti mwamuna wake atenge munda wa mpesawo , Yezebeli anakonza zakuti anthu ena akasemele mlandu Naboti ndi kupeleka umboni wotsutsana naye . Zimenezi zinacititsa kuti Naboti ndi ana ake aphedwe . Baraki anasonkhanitsa gulu lake lankhondo . Koma panali vuto linalake . ( b ) Kuyambila ca m’ma 1935 , ndi nchito ina iti imene yakhala ikucitika ? Kukonda Mulungu ndi kuopa kum’khumudwitsa , kungathandize anthu ankhanza kusintha umoyo wao , osati mwaciphamaso , koma kusinthilatu umunthu wawo . ( Yes . 6 : 11 ) Koma cifukwa ca thandizo la mzimu woyela wa Mulungu , tonse tingatengele citsanzo ca Yeremiya , amene anakamba kuti : “ Yehova ndiye coloŵa canga . Tiyeni tione zimene mabanja angacite kuti apange zosankha zovuta zimenezi mogwilizana . Anthu ena angaganize kuti popeza nkhaniyi ni yaumwini , ali na ufulu wocita ciliconse cimene akonda , malinga ngati cikumbumtima cawo ciwalola . Tikudziŵa bwanji zimenezi ? Mavuto amene amabwela cifukwa ca ngozi , kudwala , imfa ya munthu amene timakonda , ngozi za cilengedwe kapena nkhondo , zingacititse anthu kukhumudwa ndi Mulungu mosavuta . Ndinawafunsa ngati pali amene angakonde kuphunzitsidwa kuti akhale womasulila . Iwo amakonda kuyendayenda atavala mikanjo . Amakonda kupatsidwa moni m’misika ndi kukhala m’mipando yakutsogolo [ kapena kuti “ yapamwamba ” ] m’masunagoge . Amakondanso malo olemekezeka kwambili pa cakudya camadzulo . ” 1 : 8 , 9 ; Sal . 1 : 2 , 3 ) Magazini yoyamba ya Nsanja , imene inafalitsidwa mu July 1879 , inati : “ Coonadi cili ngati duŵa laling’ono m’sanga , limene lili pakati pa viudzu vimene vatsala pang’ono kuliphimba . “ Ndinali kucitila phunziloli pa nyumba pathu ndiponso pa nthawi imene ndinali kufuna . ( Machitidwe 8 : 26 - 39 ) Pambuyo pake , Mulungu anatsogolela mtumwi Petulo kukacezela kapitawo waciroma dzina lake Koneliyo amene anali kupemphela kwa Mulungu ndi kuyesetsa kum’lambila . ( Genesis 37 : 6 , 7 , 9 ) Popeza kuti malotowo anali acilendo ndi osaiwalika , kodi Yosefe akanacita ciani ? 11 : 25 , 26 . Ngakhale asayansi akopelako zacilengedwe zimenezo . Tenga ufa wosalala wokwana miyezo itatu ya seya , uukande , ndipo upange makeke ozungulila . ” Akhristu onse amafunika kukhala odzicepetsa , ndipo khalidwe limeneli limabweletsa madalitso . Dzifunseni kuti : ‘ Kodi ana anga amadziŵa cifukwa cake kuonelela zamalisece n’koipa ? Nthawi zina , timakhala ndi makonzedwe apadela a ulaliki . 2 : 7 ; Yes . 32 : 1 , 2 ) Kuonjezela pamenepo , zinthu za Ufumu zikupitabe patsogolo ngakhale kuti anthu ena akhala akutsutsa komanso kuzunza atumiki a Mulungu . — Yes . Yesu Kristu anafa kuti aombole anthu onse , ndipo zimenezi zili ndi tanthauzo lalikulu kwa anthu amene amakonda iye ndi Atate wake . ( Agal . Ndinapeza mayankho a mafunso amene anali kundivutitsa kwa nthawi yaitali . Kudzicepetsa kunathandiza wacicepele wina dzina lake Christoph kulandila uphungu . Tinalinso na mwayi kukhala ndi m’bale Frederick W . 9 : 2 Iwo anadziŵa kuti Yosefe anali mwana woyamba kubadwa kwa mkazi wake wokondedwa — amene anafunika kukwatila paciyambi . ( c ) Kodi colinga ca nkhani ino n’ciani ? Tikuitanani kuti mukapezeke pamsonkhano umenewu . Padzakambidwa nkhani imene idzafotokoza cifukwa cake imfa ya Yesu ndi yofunika . Muzitsegula mokwanila pakamwa Kale , mabuku athu anali kufotokoza kuti amuna ndi akazi okhulupilika monga Debora , Elihu , Yefita , Yobu , Rahabi , Rabeka , ndi ena ambili , anali kuimila odzozedwa kapena “ khamu lalikulu . ” 37 : 29 . ( b ) Tingaonetse bwanji kuti sitinapusitsike na cinyengo ca Satana ? Dzikoli lidzaipila - ipilabe kufikila pamene Yehova adzaliononga . Pamene Yesu anali kuyambitsa mwambo wa Cikumbutso , iye sanasinthe mozizwitsa mkate ndi vinyo kukhala thupi lake lenileni ndi magazi ake enieni . M’malomwake , muuzeni kuti mumaona makhalidwe ake abwino , ndi kuti mukudziŵa kuti amafuna kucita zabwino . Emil anayamba kukhala pafupi na mudzi wochedwa Sokuluk m’dela lathu . Koma mungadabwe kuti patsikulo , ine ndi anzanga ena tinali m’nyumba ya pa famu yosungilamo zinthu , imene munali mozizila . Koma sizinatheke . Kudzela mwa Haneni , Yehova anauza Mfumu Asa kuti : “ Maso a Yehova akuyendayenda padziko lonse lapansi kuti aonetse mphamvu zake kwa anthu amene mtima wao uli wathunthu kwa iye . ” Ngati pali ena amene ali ndi vutoli , bungwe la akulu lingakonze zakuti anthu amene amadwala cifukwa ca fungo la pelefyumu akhale paokha m’Nyumba ya Ufumu ngati n’zotheka . Cyril na Kitty Johnson anali apainiya atsopano odzipeleka kwambili . Kodi kuzindikila malo anthu m’makonzedwe a Mulungu kumaonetsa ciani ? Cifukwa cakuti anali na vuto la mtima , madokota anadela nkhawa kuti adzafa , ndipo anamunyengelela kuti acotse mimbayo . Kodi tili na udindo wanji monga atumiki a Yehova okhulupilika ? N’zimenenso iye analimbikitsa abale ndi alongo ku Roma kucita . M’Baibulo , muli zitsanzo zambili za amuna ndi akazi okhulupilika amene anali kuopa Yehova ndi kum’khulupilila , ndipo anakhala mabwenzi ake apamtima . Mwa ici , iwo sangatengeko mbali m’zocitika zilizonse zakupha anthu . ” Koma zimenezi sizitanthauza kuti ifenso tidzacila tikatsatila malangizowo . 10 Malonjezo Amene Adzakwanilitsidwa N’ndani amene ayenela kupatsidwa ulemu ? Koma kupeleka moni , ngakhale wacidule cabe , kungakhale na zotulukapo zabwino . Ife tonse timabadwa osalungama . Koma mwacionekele mu mpingowo munalinso alongo , ndipo ena anawachula maina awo . Pomalizila pake , nditawafotokozela zonse za umoyo wanga wa kale anavomela kundilemba nchito ndipo anati : “ Ndikulembabe nchito , ngakhale kuti sindikudziŵa cimene cikundicititsa kuti ndikulembe . ” DZIKO : AZERBAIJAN Kodi makolo angathandize bwanji mabanja ao kukhalabe olimba kuuzimu ? Atamufunsa ngati adzapitiliza kulalikila , iye molimba mtima anauza omunyozawo kuti : “ Ndaiganizila kwambili nkhani imeneyi . Ndingakonde kukhala m’ndende ndi kukhalabe paubwenzi wolimba ndi Mulungu m’malo mwakuti ndimasulidwe ndi kukhala paudani ndi Mulungu . ” ( Yoh . 4 : 24 ) Komabe , n’zotheka kukonda Yehova , ndipo Malemba amatiuza kuti tizim’konda . Kuti tizithandizana pa mavuto , tifunika kukhala na cifundo ceni - ceni . Nkhaniyo inafotokoza mavuto ofanana ndi amene iye anali kukumana nao . Komabe , Hans anakhalabe wokhulupilika panthawi yonse ya nkhondo . Komabe , munthu aliyense ni ‘ moyo . ’ Ni maganizo olakwika ati amene anthu ena angakhale nawo pa macimo awo ? ( Yes . 43 : 21 ; 44 : 26 - 28 ) Pamene anthuwa anabwelela kukamanganso kacisi wa Yehova ku Yerusalemu , anakhala mboni pankhani yakuti Yehova , Mulungu yekha woona , amakwanilitsa mau ake nthawi zonse . Kaya ndimwe kholo kapena ayi , mufunika kusankha mabwenzi anu mwanzelu . “ Cimakhala copepuka kukhululukilana ngati nonse aŵili mwalakwitsa , koma cimakhala covuta ngati mmodzi ndiye walakwitsa . Yehova satisankhila mayeselo amene timakumana nawo . Koma kumbukilani citsanzo ca munthu wina dzina lake Yobu . Kuti timvetsetse kusiyana kwake , tiyeni tiyelekezele motele : Tinene kuti mwaima pakati pa mseu , ndipo kutsogolo kukubwela basi . Coyamba , mwazindikila kuti galimoto imene ikubwelayo ndi basi . Komabe , Baibo imakamba kuti Yosefe anali “ munthu wabwino ndi wolungama . ” 2 : 4 ) Kodi inu mungam’thandize bwanji mwana wanu kupewa vuto limeneli kuti ‘ akule ndi kukhala oyenela cipulumutso ’ ? ( 1 Pet . Nthawi zakale , sizinali zodabwitsa kuona mau ozokotedwa pa maziko a nyumba oonetsa amene anaimanga kapena mwiniwake . Kodi tingamutsanzile bwanji Yesu pankhani yoganizila madalitso amene timapeza cifukwa copilila ? Pamene kabokosiko kanadzala , anapeleka ndalamazo kuti zithandizile pa nchito yolalikila . ( Luka 4 : 1 - 13 ) Ngati timacilikiza ulamulilo wa Mulungu ndi kum’khulupilila , palibe aliyense angaticititse kuti tipeputse malamulo ake . Pali zifukwa zambili zokondela Yehova . Kodi Anna analibe mwai wotani ? Nanga anacita ciani kuti atumikile Mulungu ? Mulungu Wosaonekayo Mungamuone ? — July - August Tikamagwilizana ndi abale amenewa , timathandiza kuti zinthu ziziyenda bwino komanso mwadongosolo mumpingo . — Yelekezelani ndi Machitidwe 6 : 3 - 6 . Masiku ano , pali zinthu zambili zimene zingatisokoneze kutumikila bwino Yehova . PA DZIKO lonse , zipembedzo monga Chechi ya Roma Katolika , machechi osiyana - siyana a Orthodox , Cibuda , ndi zipembedzo zina , zimafuna kuti azibusa ndi atsogoleli awo azikhala osakwatila . COLINGA CA MOYO Kodi abale athu anali okangalika mu nchito yolalikila m’nthawi ya nkhondo yoyamba ya pa dziko lonse ? Koma masiku ano pali Mboni za Yehova pafupifupi 8 miliyoni . Mwina imwe munataikilidwa wokondedwa wanu , kapena mudziŵako munthu wina amene anafedwa . Zinthu sizinali bwino kwa ine . ” Ndithudi , Atate wathu wakumwamba timamukonda ndi mtima wonse , potipatsa ciyembekezo cimeneci . Fanizolo limatha ndi mau akuti : “ Iwowa [ amene ali ngati mbuzi ] adzacoka kupita ku cionongeko cothelatu , koma olungama ku moyo wosatha . ” — Mat . Kwa zaka zambili , zofalitsa zathu zakhala zikufotokoza mafanizo a Yesu mwa njila yomveka bwino . M’caputa 3 timaŵelenga kuti : “ Onse ndi ocimwa ndipo . . . kuyesedwa olungama cifukwa ca kukoma mtima kwake kwakukulu kumene wakusonyeza , powamasula ndi dipo lolipilidwa ndi Khiristu Yesu , kuli ngati mphatso yaulele . ” Conco , ndi pofunika kumvela cenjezo la Yesu lakuti : “ Koma samalani kuti mitima yanu isalemedwe ndi kudya kwambili , kumwa kwambili , ndi nkhawa za moyo , kuti tsikulo lingadzakufikileni modzidzimutsa ngati msampha . ” ( Luka 21 : 34 , 35 ; Chiv . Mbili imasonyeza kuti mfundo za makhalidwe abwino zikalowa pansi , mabungwe ndi maboma amagwa . Liu la Ciheberi limene analitembenuza kuti ‘ kugalamuka ’ limatanthauza “ kubwatama ” kapena “ kuŵila . ” Goliyati ananyoza Yehova Mulungu , ndipo Yehovayo anacitapo kanthu . Aroni amaimila Yesu Kristu , ndipo ana ake amaimila otsatila odzozedwa a Yesu . Liu la Cigiriki lomasulidwa kuti ‘ kuphunzitsa anthu ’ pa Mateyu 28 : 19 , limatanthauza kuphunzitsa na colinga copanga ophunzila . M’kupita kwa nthawi , ena a m’banjalo anacitanso cimodzi - modzi . Ngati mwaona kuti ana anu sakonda kwambili utumiki , athandizeni kuyamba kusangalala ndi utumiki . ( a ) Kodi acicepele apindula motani ndi Kulambila kwa Pabanja kokhazikika ? 11 , 12 . Idzatithandiza kuyamikila mwai wathu wogwila nchito ndi Mulungu , umene tiyenela kuyamikila kwambili . Kodi Baibulo linali litamasulidwa m’zinenelo zingati podzafika m’caka ca 1900 ? Ndiyeno , mofanana ndi alambili a Yehova akale , tifunika kupitiliza kusinkha - sinkha malonjezo a Mulungu ndi kumvela malamulo ake . ( 1 Mbiri 3 : 17 ; Mateyu 1 : 12 ) Zikuoneka kuti Salatiyeli anakwatila mwana wamkazi wa Neri amene sanachulidwe dzina . Motelo , iye anakhala mpongozi wa Neri . Ndipo anavomela kuyamba kuphunzila Baibo na M’bale John E . Conco , mofanana ndi Yoswa , tifunika kumaŵelenga Mau a Mulungu na kuwaseŵenzetsa . Zimene mungacite ngati mulibe mnzanu Atumiki ambili a Mulungu , amuna ndi akazi , odzozedwa ndi a khamu lalikulu , akumanapo ndi mavuto monga a Yobu , ndipo ‘ aona zimene Yehova anamupatsa , aona kuti Yehova ndi wacikondi cacikulu ndi wacifundo . ’ — Yak . M’zaka zimenezo , panali anthu ena okhulupilika amene anali kufuna kudziŵa coonadi ndi kutumikila Mulungu ngakhale kuti ziphunzitso zonama zinali zofala . N’cifukwa ciani pamafunika khama kuti tikhale auzimu na kuteteza uzimu wathu ? Cikumbumtima cake citamuvuta , anauza Farao kuti iye ndi mkulu wa ophika mkate analota maloto m’ndende zaka ziŵili zapitazo , ndipo mnyamata wina wanzelu amene ali m’ndendemo anamasulila malotowo . Ndinali kuŵelenga Baibulo , koma sindinali kulimvetsetsa . Mwina tingayambe ( 1 ) kudalila nzelu za anthu mosadziŵa , ( 2 ) kugwilizana ndi anthu oipa , ( 3 ) kudzikuza , kapena ( 4 ) kupanga zosankha tisanaganizile zimene Mulungu afuna . Cifukwa cakuti simudziŵa mmene anzanu angalandilile uthenga wanu . Timapindula bwanji tikamakambilana za ciyembekezo cathu ? N’natumanso foni kwa m’bale Marais kumuuza kuti ndife okonzeka kucita utumiki wapadela umenewu . Sukuluyo inali pamtunda woyenda maola angapo kucokela kumene kunali kukhala banja lathu . ( Sal . 40 : 17 ) Nthawi zambili , Yehova monga Mpulumutsi , amapulumutsa anthu ake monga gulu maka - maka pamene akuzunzidwa mwakhanza ndi adani ao . 1 : 26 , 27 ; 2 : 3 ) Pamene Paulo anakamba za anthu amphamvu , sanali kutanthauza kuti Akristu amenewo ayambe kudziona apamwamba . Cifukwa coyamba n’cakuti timatengela citsanzo ca Yesu , amene ‘ sanali mbali ya dziko . ’ Kodi mayendedwe osavuta anathandiza bwanji Akristu panchito yao yolalikila ? Nanga cinenelo ca Cigiliki cinawathandiza bwanji ? Kodi cilako - lako cofuna kukhala wodziŵika kwa ena cingatisoceletse bwanji ? Anthu a Yehova padziko lapansi adzasangalala na zinthu zambili zabwino . Nkhani ino , idzatikumbutsa citsanzo cabwino cimene Yefita ndi Hana anatipatsa pamene tiyesetsa kukwanilitsa zimene tinalonjeza kwa Mulungu . 5 : 14 , 15 . Ngati ndi conco , kodi muyenela kucita ciani ? Kodi inu mudzamuonetsa bwanji Yehova kuti mumam’konda ? Ganizilani zitsanzo ziŵili izi : Ku Korea , pa Mboni 100 zomwe ndi mbeta , 57 ndi alongo , ndipo 43 ndi abale . 8 : 31 . 15 : 4 - 6 ) Kunyada ndi kumene kunacititsanso kuti Kaini acimwe . ( 3 Yohane 4 ) Ngakhale n’conco , atumiki anthawi zonse amacita zimene angathe ngati makolo ao afunikila cisamalilo . Iye anati : “ Nikanapanda kulola Yehova kunithandiza kuvula umunthu wakale ndi kuvala watsopano , sembe sin’nakwanitse kukhala na makhalidwe abwino amenewa . ” Paulo anayenda m’madela ambili komanso akutali , monga ku dziko limene lomba limachedwa Turkey , ku Greece na ku Italy . ( Eks . 32 : 14 ) Mose ataona zinthu zonyansa zimene anthuwo anali kucita , monga kukuwa , kuimba , na kuvina patsogolo pa fano , anatenga mwana wa ng’ombeyo na kumuphwanya - phwanya mpaka kukhala fumbi lokha - lokha . Zikumbutso za Yehova ndi zodalilika , zimapatsa nzelu munthu wosadziŵa zinthu . ” Ngati mwamuna ndi mkazi amakonda Yehova ndi kum’tumikila , banja lao limakhala lacimwemwe ndi logwilizana Hannah ndi mwamuna wake , Patrick , atumikila ku Majuro pazilumba za Marshall . Yesu sanacimwepo kapena kuphwanya lamulo limodzi la Mulungu , ngakhale atakumana ndi mayeselo aakulu kwambili . Anazunzidwa cifukwa ca ife kuti tidzakhale ndi moyo wosatha . 6 : 32 . Iye anauza Yesu kuti akamulambila kamodzi kokha cabe , adzakhala mfumu pa nthawi imeneyo . Iwo amaganiza kuti kungokhala munthu wabwino n’kokwanila kuti ukondweletse Mulungu , mosasamala kanthu za cipembedzo cako . Mizinda 6 yothaŵilako inali yosavuta kufikako . 2 : 22 ) Panthawi imeneyo , Timoteyo anali wamkulu kale , mwina anali ndi zaka za m’ma 30 . Poyankha Yesu anati : “ Amene waona ine waonanso Atate . ” N’zosatheka kukhala ku mbali zonse ziŵili pa nthawi imodzi . Khalani oona mtima . Tiyamikila kuti tinatsatila malangizo a mu Utumiki Wathu wa Ufumu ndi kudalila Yehova . ” ( Luka 1 : 78 ; 2 Akor . 1 : 3 ; Afil . “ Limbani m’cikhulupililo , . . . khalani amphamvu . ” — 1 AKORINTO 16 : 13 . Cimaya ndi cimodzi mwa zinenelo zimenezo . Pambuyo pobwezeletsedwa mu mpingo , m’bale wina amene anatengeka na cilokolako coipa mpaka kucita ciwelewele , anakamba kuti : “ N’nasoceletsedwa kwambili na zilakolako zoipa cakuti panatenga nthawi itali kuti nibwelele mu mpingo . ” Koma limapelekanso cifukwa cake samamvetsela mapemphelo ena . Zimenezi zimabweletsa magaŵano mumpingo . Lefèvre anabwadwila m’banja la Akatolika ndipo anali kuona kuti chechi cingapite patsogolo kokha ngati anthu wamba aphunzitsidwa bwino Malemba ndi kuwamvetsetsa . Kumeneko anawapatsa kaufulu kocitako zinthu zaumwini , ndi kuyenda kulikonse kumene anafuna m’dzikomo . Patapita nthawi yocepa ndili ku Austria , ndinapeza nchito . 17 : 16 ) Yehova analosela kuti tidzakhala ngati anthu opanda citetezo , monga ‘ midzi yopanda mipanda . . . ilibe zotsekela ndiponso zitseko . ’ ( Ezek . Yesu anagonjetsa imfa . NYIMBO : 60 , 135 Nthawi ina , n’napelekeza M’bale Finch pa ulendo wake wokalalikila kumpoto kwa dziko la Pakistan . ( Aefeso 5 : 15 , 16 ) Conco , m’malo motumila ena zinthu zimene sitinatsimikize kuti n’zoona , zingakhale bwino kuganizila mwakuya kuti : “ Ngati ndikaikila , ndiye kuti ndiyenela kupewa kutumizila ena zinthu zimenezi . ” Njila yaikulu imene timamvetselela kwa Yehova ni mwa kucita phunzilo la Baibo laumwini . Ngati n’conco , mungalimbikitsidwe ndi citsanzo ca Paulo . Ndili ku Madrid , ndinalumbila kaciŵili kuti ndikhale sisitele . Pamene tipitiliza kubala zipatso mopilila , timakhala pa ubwenzi na Yesu . 51 : 12 ; 54 : 6 ; 110 : 3 . Nanga Mau a Mulungu amaphunzitsanji pa nkhani yopeleka moni ? ’ Paulo anali kudziŵa kuti cikondi ca Mulungu siciyang’ana nkhope , komanso Iye salekelela zolakwa . Amatifika pamtima ndi kutilimbikitsa kugwilitsila nchito zimene timaphunzila . — Akol . NYIMBO : 43 , 106 13 CITSIMIKIZO CAMPHAMVU KUCOKELA KU KACILEMBO KOCEPETSETSA KACIHEBERI “ Mtendele wa Mulungu . . . Tidziŵa bwanji kuti Mau a Mulungu alidi na mphamvu ? Nkhani ina m’magazini yochedwa Monitor on Psychology inati : Vuto ni “ kufunitsitsa [ ndalama ] n’kumene kumalengetsa munthu kusakhala wacimwemwe . ” “ Kusukulu , tonse tinali kufunika kupeleka pemphelo loloweza pamtima limene tinaphunzitsidwa . ” — Teresa , wa ku Philippines . Anthu a m’tauni ya Aue anayamikila kwambili khama langa cakuti akulu - akulu a boma ananipatsa mphoto . N’zoona kuti nthawi zina tingasiyane maganizo pankhani zing’ono - zing’ono ndi okhulupilila anzathu . Ni chimo lanji limene Yesu anali kukamba pa Mateyu 18 : 15 - 17 ? Yehosafati anacita mantha . Popeza kukhala waubwenzi kumatanthauza kulankhula ndi ena komanso kuwamvetsela akamalankhula , muzionesetsa kuti mumacita cidwi ndi anthu ena . Kamodzi iye anaonekela kwa khamu la anthu oposa 500 . Otsatila a Yesu naonso anali kupeleka zimene angakwanitse . Ndinadziŵanso kuti kupanduka kwa Adamu ndi Hava kunabweletsa mavuto pa mtundu wa anthu . ( Yer . 27 : 11,12 ) Patapita zaka 70 , anthu a Mulungu amene anali kumeneko anaonako pamene ulosi wodabwitsa unakwanilitsidwa wakuti : “ Yehova , Wokuombolani , Woyela wa Isiraeli wanena kuti : ‘ Cifukwa ca inu , ndidzawatumiza ku Babulo . Ndidzacititsa kuti zitsulo za ndende zimasuke . ’ ” — Yes . Aisiraeli amene anayamikila mwai wodziŵika ndi dzina la Yehova , mwacionekele anauzako ana ao ndi alendo amene anali akapolo ao , zinthu zimene Mulungu anacita . Koma chalichi cimene amapitako cinali kundidabwitsa . Pamene Yesu anali padziko , anaonetsa kuti ni Woyenela kukhala Mfumu . Onani kuti Paulo pochula makhalidwe oipa amene adzakhala ofala m’masiku otsiliza , anayambila kuchula khalidwe la kudzikonda . Akatswili ena a Baibo amakamba kuti iye anatelo cifukwa makhalidwe enawo amayamba cifukwa ca kudzikonda . Pambuyo pake , Mulungu sanalolenso mbadwa iliyonse ya Eli kutumikila monga mkulu wa ansembe . Nimakumbukilabe nkhani imene iye anakamba , ya mutu wakuti , “ Ni M’mbuyo mwa Alendo ! ” Kwa amene amacita zimenezi , ‘ mphamvu zawo zidzapitiliza kuwonjezeka . ’ N’ciani cinacitikila Gehazi cifukwa ca zimene anacita ndi kunama bodza kwa Elisa mneneli wa Yehova ? “ Tamandani Ya . . . pakuti kuimbila Mulungu wathu nyimbo zomutamanda n’kwabwino . ” — SAL . Mwacitsanzo , Yehova amatilangiza kuti tifunika ‘ kuleka kuyanjana ’ ndi anthu ocita zoipa amene safuna kulapa . Yehova walonjeza kuti adzakhala ku mbali yathu . Khalidwe limeneli n’logwilizana ndi mau a Paulo akuti “ ndife ziwalo za thupi limodzi . ” ( Aef . Pamene tisinkhasinkha za makhalidwe a Yesu a kudzicepetsa ndi cifundo , timalimbikitsidwadi kupitiliza kutsatila mapazi ake . Mlongo wina dzina lake Berenice ali ndi ana anai , ndipo onse anabatizidwa asanafike zaka 14 . Munthu wodzicepetsa amaganizilanso mmene zocita zake zingakhudzile anthu ena . Popeza kuti timakhala otangwanika ndi nchito za masiku onse , sitidziŵa kuti mbeu za coonadi zikukula . Tiyeni tikambilane njila ziŵili . Kusiyana pakati pa anthu amene amatumikila Mulungu na amene sam’tumikila kukuonekela ngako tsopano . Fotokozani zimene Yesu anacita asanakumane ndi munthu wolemala ku Yerusalemu . Akulu ali “ ngati malo obisalilapo mphepo ndi malo ousapo mvula yamkuntho , ngati mitsinje yamadzi m’dziko lopanda madzi , ndiponso ngati mthunzi wa thanthwe lalikulu m’dziko louma . ” ( Yes . Ngakhalenso m’mitima yathu tinali kumva ngati talandila ciweluzo ca imfa . Yobu wa m’nthawi yakale anali ndi cocitika cofanana . Kodi Yehova waonetsanso bwanji kuti amavomeleza kuphunzitsa m’njila yosavuta ndi yomveka bwino ? Zimenezi zidzacititsa kuti ambili ayambe utumiki wa nthawi zonse ndi kuti akhale “ oyenelela bwino kuphunzitsa . ” — 2 Tim . ( Yes . 25 : 6 - 9 ; 65 : 21 , 22 ) Koma pali pano , otsatila a Yesu afunika kucita zinthu “ mwanzelu ” pogwilitsila nchito “ cuma cosalungama kuti apeze zofunikila pa umoyo . ” Iye analemba kuti : “ Timakumbukila nthawi zonse nchito zanu zacikhulupililo , ndi nchito zanu zacikondi . Timatelonso pokumbukila mmene munapililila cifukwa ca ciyembekezo canu mwa Ambuye wathu Yesu Kristu , pamaso pa Mulungu wathu ndi Atate . ” Yesu anali atangoŵauza kumene kuti iye ndi mfumu . Mwina Yesu sanali kuyembekezela kulandila mphatso imeneyi cifukwa cakuti moyo wosafa suchulidwako paliponse m’Malemba Aciheberi . Mwacitsanzo , mvelani zimene zinacitika ku Japan . ZIFUKWA ZIMENE ENA SAFUNILA KUGAŴILA ENA MAUDINDO Zimene anakamba zionetsa kuti anali munthu wokonda kwambili Mau a Mulungu , ndipo anali kuwadziŵa bwino Malemba Aciheberi . ( Gen . 30 : 13 ; 1 Sam . 2 : 1 - 10 ; Mal . Otsalila a odzozedwa amayamikila kwambili ‘ anamwali anzao ’ amenewa cifukwa cakuti amacita khama pa nchito yolalikila “ uthenga wabwino uwu wa ufumu ” padziko lonse lapansi . ( Mat . Ngakhale kuti sitidziŵa zonse , Mulungu watiuza zambili za mmene umoyo udzakhalila mu Ufumu wake umene ‘ timayang’anitsitsa . ’ Tsiku lotsatila , Ophunzila Baibo anakwela boti ya melo kupita ku Liverpool . Kumeneko , anakwela sitima ya pamadzi yochedwa Lusitania kupita ku New York . Musaleke kutumikila Yehova cifukwa cakuti wina anakukhumudwitsani . Cikondi ca Yehova pa anthu ndi ciyembekezo cimene wawapatsa zinandicititsa kuti ndilekeletu cizoloŵezi cimeneci . ” Ndipo analenga anthu m’cifanizilo cake . Tikayenda ku msonkhano , timadziŵa nthawi imene mapulogilamu adzayamba . Abale ndi alongo odzimana amenewa amathandiza kwambili pa nchito yokolola mwa kuuzimu . Sanatope ndi nchito yao kapena kungoileka , koma anaigwilabe mpaka kumapeto . Tsiku lililonse timayandikila nthawi imene Ufumu wa Mulungu udzabwela . Ufumuwo ukadzabwela , padziko padzakhala mtendele , ndipo anthu onse adzakhala angwilo . Mwamuna wina wofedwa anati : “ Ine ndi mkazi wanga sitinafune kuti cikwati cathu cithe . Patapita pafupi - fupi caka cimodzi kucokela pamene Lefèvre anathaŵa , Mfumu Francis Woyamba anamusankha kuti aziphunzitsa mwana wake wa zaka 4 , dzina lake Charles . Analinso ndi “ ana aamuna ndi aakazi , ” koma ciŵelengelo cawo sicidziŵika . Kuyambila m’caka ca 1914 , kodi zocitika za padziko lapansi zikukwanilitsa bwanji ulosi wa m’Baibo ? Ngakhale pakati pa Akhristu ena oyambilila panabuka mikangano . Ndiye cifukwa cake Yakobo anawafunsa kuti : “ Kodi nkhondo zimene zikucitika pakati panu zikucokela kuti ? ” Kodi akatswili ofufuza zinthu zakale apeza umboni uliwonse wosonyeza kuti mzindawo unagonjetsedwa m’nthawi yocepa , monga mmene Baibulo limanenela ? Iwo anali pafupi kukumana ndi ciyeso cacikulu kwambili . Koma Yesu anakamba kuti Atate ŵake amayang’ana anthu amene amacitila anzawo zabwino , olo kuti anthu ena sanaone . Kwa zaka zambili , m’maiko monga Congo , Madagascar , ndi Rwanda , Mabaibo anali odula ngako cakuti mtengo wake unali kulingana ndi malipilo amene munthu woseŵenza anali kulandila pa wiki kapena a pa mwezi . Kumeneko ndinakwatila mkazi wokongola dzina lake Jenny Alcock , ndipo tinatumikila ku tauni ya Smithton ndiponso ku Queenstown kwa zaka 4 monga apainiya apadela . Ciukililo cofunika kwambili pa ziukililo zimenezo ni ca Yesu . Iye afuna kuti tikhale anzelu , okondwela , ndi kuti tizimukonda monga Atate wathu . Gerald Grizzle Pamene aona zimene ise makolo timacita mu umoyo , zimakhala monga kuti nthawi zonse akuphunzitsidwa . ” — Wendell . Riana ni m’bale wa zaka za m’ma 20 . Conco , sin’nakhulupilile zimene anacita . 3 : 12 ) Cinanso , ngakhale kuti iye na Yosefe anali atakwatilana kumene , sanakhaleko malo amodzi mpaka Yesu atabadwa . 1 : 37 ; 3 : 26 ) N’cifukwa ciani anakwiya ? Panthawi imeneyi , ndinali wacisoni kwambili ndi kumwalila mwadzidzidzi kwa atate anga , ndiponso cifukwa ca mavuto ena apabanja lathu . Uthenga umenewo uyenela kuti udzaphatikizapo uthenga wakuti dziko la Satana lili pafupi kuonongedwa . Gulu la Yehova likuyesetsa kuthandiza pa nchito yomanga Nyumba za Ufumu kulikonse kumene zikufunika . ( Aroma 5 : 12 ) Baibulo limati : “ Mulungu akuonetsa cikondi cake kwa ife , moti pamene tinali ocimwa , Kristu anatifela . ” 1 , 2 . ( a ) Kodi tingalimbikitsidwe bwanji na citsanzo ca Nowa , Danieli , na Yobu ? Koma mosayembekezela , tinalandilanso utumiki watsopano . 2 : 24 ; 1 Akor . 7 : 39 ) “ Conco , ” mogwilizana ndi mau a Yesu , “ cimene Mulungu wacimanga pamodzi , munthu asacilekanitse . ” Ndimeyi ifotokoza zimene zinali kucitika kale - kale m’ndende zina ku United States . Pamapeto pake , Mulungu analeka kumuyanja na kum’cilikiza . A Daka : N’zoona . 12 : 9 ) Koma sitiyenela kumuyopa maningi Mdyelekezi , cifukwa mphamvu zake zili na pothela . Panthawi ya nkhondo m’caka cimeneco , Akristu odzozedwa masauzande ocepa , amene ndi “ ana a Ufumu , ” anali mu ukapolo wa kuuzimu wa Babulo Wamkulu . Hana anali kutonzedwa na Penina “ caka ndi caka . ” N’cifukwa ciani atumiki a Yehova anafunika kuwongoleledwa na kupatsidwa cilangizo pa nthawi ya nkhondo yoyamba ya dziko lonse ? Mufunika kuika maganizo anu pa zimene muŵelenga ndi kuganizila tanthauzo lake . Amuna 40 analemba Baibulo mouzilidwa ndi Mulungu . Ngati Mkristu wadzozedwa , kodi zikutanthauza kuti basi adzapita kumwamba ? M’dziko latsopano , sitidzaopanso mvula yamkuntho , tsunami , kuphulika kwa mapili , kapena zivomezi . Sikuti anacita cidwi ndi mapalewo cabe , koma ndi mau amene analembedwapo . • “ Yehova ndi wacikondi cacikulu ndi wacifundo . ” — Yakobo 5 : 11 . Koma bwanji ngati talakwa . N’cifukwa ciani tifunika kucita zilizonse zimene tingathe pamene tikulalilkila m’masiku otsiliza ano ? Komabe , panthawi ina anakhumudwa kwambili cakuti anapempha Yehova kuti afe . Iye anati : “ Basi ndatopa nazo . ( Chiv . 2 : 10 ) Ndipo Akristu ena okhulupilika akuyembekezela kudzakhala ndi moyo wosatha m’Paladaiso padziko lapansi . Cimapeleka mphamvu zothandiza mabwenzi na mabanja kupilila Buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu akuligwilitsilanso nchito pocita ulaliki wapoyela . Pali colinga cimene anthu ena amapitila kumwamba . Wokwela pa hosi yacinayi akuimila imfa imene ikucitika cifukwa ca milili ndi zinthu zina . Yehova anamulonjeza kuti : “ Ndidzakupatsa moyo wako monga cofunkha cako . ” ( Yer . Kodi masomphenya otsilizila a Zekariya anawatsimikizila ciani anthu a Mulungu ? Koma Yehova Mulungu anan’thandiza kuti nipambane nkhondoyo . — Salimo 55 : 22 . Pamene Petulo ndi atumwi ena anaikidwa m’ndende ndi kumenyedwa cifukwa colalikila , io anakondwa “ cifukwa cakuti Mulungu anawaona kuti ndi oyenela kucitilidwa cipongwe cifukwa ca dzina la Yesu . ” ( Mac . Kucita zimenezi kudzaonetsa kuti ndise odzicepetsa ndipo ‘ timaona ena kukhala otiposa . ’ ( Afil . Anali kudzifunsa kuti , ‘ Nisamalila bwanji banja langa ? Kodi cikumbumtima canu cimakulimbikitsani kucita zabwino ? Yesu anati : “ Pitilizani kufunafuna ufumu coyamba ndi cilungamo cake , ndipo zina zonsezi [ kuphatikizapo zakudya , zakumwa , ndi zovala ] zidzaonjezedwa kwa inu . ” Malangizo amene timapatsidwa pampingo amatithandiza kuti ticite zimenezi . ( b ) Kodi Adamu ndi Hava anasankha ciani ? N’zotheka kuti inunso mumamva mmene Sarie , mlongo wa ku South Africa , amamvelela . Iye wakhala akucitila umboni mokangalika kwa zaka zopitilila 60 . M’malomwake , panthawi imeneyi , yesetsani kupita patsogolo mwakuuzimu kuti muyenelele ubatizo . 4 Mungayambe Bwanji Kuŵelenga Baibo ? Pa nthawi ina , Mfumu Davide atacita chimo , anazunzika na cikumbumtima cake . Anthu oipa akamacitila nkhanza anthu osalakwa , zimatipweteka mtima kwambili . 5 : 9 , 10 . Maria ali ndi ana athu , Olga ndi Irina , mu 1965 ( Zefaniya 2 : 3 ) Motelo , sitifunika kutsatila gulu la anthu ndi kunyalanyaza zizindikilo zoonetsa kuti tili m’masiku otsiliza , m’malomwake ‘ tizikumbukila nthawi zonse kukhalapo kwa tsiku la Yehova . ’ Komabe , Yehova amatipatsa zikumbutso za panthawi yake ndi thandizo loyenelela kuti titetezedwe ku zinthu zimene zingaononge ubwenzi wathu ndi iye . M’bale amene “ akuyesetsa kuti akhale woyang’anila , ” kapena kukhala ndi maudindo ena m’gulu la Yehova amayamikila mau olimbikitsa . ( 1 Tim . Tinali kufuna kusiila ana athu zitsanzo zabwino zimene tinatengela kwa ena . Kodi mungakonde kuphunzila zambili ? ? Sindidzaiŵala zimene ndinakambilana ndi wansembe wina . Cifukwa cakuti Mose anali kukhulupilila ndi kumvela Yehova . Iye ‘ sanaope mfumu ayi , pakuti anapitiliza kupilila moleza mtima ngati kuti akuona Wosaonekayo . ’ — Ŵelengani Aheberi 11 : 27 , - 28 . Bwanji osakonza zakuti tsiku lililonse muziganizila zinthu zosacepele zitatu zimene mungamuyamikile Mulungu ? Ngati n’conco , dzifunseni kuti , ‘ Kodi kusamukila mumpingo umenewu kudzanithandiza kukhala pa ubwenzi wolimba na Yehova ? ’ Mwa kusankha kukonda Mulungu , kumumvela , na kum’mamatila , ndiye kuti mukusankha kukhala na moyo . Inde , moyo wosatha m’paradaiso padziko lapansi . Mu June 1951 , onse aŵili anabatizika , ndipo anayamba upainiya pambuyo pa miyezi 6 . ( Tito 2 : 12 ) Zimenezi n’zofunika kwambili makamaka ngati njila zopimila matenda kapena cithandizo ca mankhwala n’zokaikitsa . Kuti tipambane pankhondoyi , tifunika kulimbana naye ndi kukhala olimba m’cikhulupililo . ( Aroma 8 : 22 ) Kodi muganiza kuti Mulungu amamva bwanji akaona anthu akuvutika ndi mavuto obwela ndi ucimo ? Yosefe sanagonje pamene mkaziyo anali kumunyengelela . Mandy ananionetsa maulosi enanso a m’Baibo okhudza tsogolo lathu . Abulahamu anauza Eliezere kuti ndiye adzatenge coloŵa iye akadzafa . Mwacionekele , iye sanatanthauze kuti mtumiki wa Mulungu sadzakhala ndi nkhawa iliyonse . Munthu aliyense ayenela kupanga cosankha ca mmene adzagwilitsila nchito umoyo wake monga mmodzi wa Mboni za Yehova . Nthawi zambili anali “ kupaka phula malo olumikizana ndipo ngakhale kunja konse kwa ngalawa , ndi mkati momwe anali kupakamo phula . ” ( Aroma 1 : 20 ) Koma kuti tim’dziŵe bwino Mulungu , tifunikila kuphunzila Mau ake , Baibo . Koma dziŵani kuti m’Malemba , mulibe pamene paonetsa kuti Yosefe anauzako munthu wina aliyense zakuti abale ake ndiwo anam’gulitsa . Ngakhale Farao sanamuuze . Mtumwi Paulo anati : “ [ Mulungu ] amapatsa anthu onse moyo , mpweya , ndi zinthu zonse . 65 : 17 . Mofananamo , Baibulo limatiuza kuti m’dziko latsopano tidzalandila mipukutu ya malangizo atsopano . 3 Yehova Amatiumba Yesu anatipatsa malangizo abwino kwambili amene angatithandize kupeza zinthu zofunika mu umoyo popanda kucenjenekwa , kukonda zinthu zakuthupi kapena kukhala ndi nkhawa kwambili . Ofalitsa ambili amakonda kuuza anthu ena za webusaiti yathu ya jw.org . Pa webusaiti imeneyi anthu angaŵelenge ndi kutenga zofalitsa zofotokoza Baibulo m’zinenelo zoposa 700 . Timakhalanso tikugwila nchito limodzi ndi angelo , amene akuthandiza anthu a Mulungu kulalikila uthenga wabwino . — Chivumbulutso 14 : 6 . 95 : 2 ; 100 : 4 , 5 ) Anthu ambili amaganiza kuti tiyenela kupemphela cabe ngati tifuna zinthu zinazake kwa Mulungu . 51 : 1 . Timalakwa tsiku lililonse . Kukhala na cizoloŵezi cocita zinthu zauzimu kungakuthandizeni kuti mukhalenso na maganizo oyenela , ndiponso kuti musamakhale na nkhawa kwambili . Anthu kapena magulu a anthu amene amapanga gulu la okana Kristu amafalitsa mabodza . Kodi tiyenela kuonetsa cifundo nthawi zonse ? Akhristu okwatilana amene akuganiza zoseŵenzetsa njila ya cilezi imeneyi angacite bwino kufunsila kwa madokota za mtundu wa ma IUD amene alipo m’dela lawo . Baibulo limakambanso kuti Yehova amasangalala kwambili ngati ticita zimene tingathe kuti tim’tamande , ndipo afuna kuti tizim’tumikila mosangalala . ( 1 Mbiri 28 : 11 – 29 : 5 ) Mofananamo , mungacite zilizonse zimene mungakwanitse kuti muthandize pa nchito imene ikucitika m’gulu la Yehova padziko lonse . Kodi anthu amene ali na “ mtima wosweka ” mungawatonthoze bwanji ndi kuwalimbikitsa ? ( Miy . Ndine wokondwela kwambili kuti sindinapite nao . NKHANI YA PACIKUTO | N’CIFUKWA CIANI TIYENELA KUPEMPHELA ? Akhozanso kuwathandiza mwauzimu . ( b ) N’cifukwa ciani tifunika kuiona kukhala yofunika kwambili ? Panthawi ina , Yesu anapempha Yehova kuti ateteze ophunzila ake . Ndinaphunzila Kulemekeza Akazi ( J . Tiyelekezele motele : Mwana akayamba kuphunzila kuyendetsa njinga , kholo lake limagwilila njingayo kuti asagwe . Iye ni “ wacifundo ndi wacisomo , wosakwiya msanga ndiponso wodzaza ndi kukoma mtima kosatha ndi coonadi . ” 10 ) Komabe , nthawi zina kupewa kugwilizana ndi wocotsedwa kumakhala kovuta cakuti kumaoneka ngati n’kosatheka . ( Genesis 37 : 4 ; 45 : 4 , 5 ) Kuganizila citsanzo cimeneci kuyenela kuti kunamuthandiza kucita zinthu zokondweletsa Yehova . Timadziŵa zimenezo cifukwa ca zimene iye anakamba kuti : “ Ndimalankhula zinthu izi ndendende mmene Atate anandiphunzitsila . ” ( Yoh . ( Mateyu 1 : 6 - 16 ; Luka 3 : 23 - 31 ) N’zoonekelatu kuti Davide anali munthu weni - weni . Mtumwi Paulo anatomola mtendele monga khalidwe lacitatu pa makhalidwe “ amene mzimu woyela ” umabala . Ophunzila Baibulo anayamba kuchedwa Mboni za Yehova mu 1931 . — Yes . Paulo anaonjezela kuti : “ Mulungu anacita izi pofuna kuonetsa cilungamo cake pokhululuka macimo amene anacitika kale . ” Anthu a m’dzikoli amadzionetsa monga olambila Mulungu , koma zocita zawo sizionetsa kuti amam’lambiladi . Iye anati : “ Iwo anandionetsa dzina la Mulungu woona m’Baibulo , kuti ndi Yehova . Kuphunzila Malemba mwakhama , kupezeka pamisonkhano nthawi zonse ndi kutengamo mbali m’nchito yolalikila zinali zofunika kwambili . Mu Isiraeli munali mizinda 6 yothaŵilako . Koma pamene mwanayo akula , apitilizabe kuganizila funsolo . N’nayamba kuphunzila naye Baibo , ndipo anapita patsogolo mpaka kubatizika . Kodi tingakambe kuti nkhani za m’Baibulo zimakhala ndi mfundo zothandiza cabe , ndipo zilibe matanthauzo ena ? 23 Kodi Mudzatengelapo Phunzilo pa Zimene Zinalembedwa ? ( 1 Sam . 16 : 13 ) Amuna onsewa anadalila mzimu wa Mulungu kuwathandiza . Ndipo mzimuwo unawathandiza kucita zinthu zazikulu zimene sakanazikwanitsa mwa mphamvu zawo . ( Yos . 11 : 16 , 17 ; Ower . 7 : 7 , 22 ; 1 Sam . N’cifukwa ciani munthu amene anali wodzicepetsa anakaniwa na Mulungu ? 1 : 4 - 28 ) Yehova ndiye akuyendetsa galeta imeneyi , ndipo imapita kulikonse kumene mzimu wake waitsogolela . Ndinakumana ndi mlongo wina wokongola dzina lake Lidasi amenenso anakulila m’banja la Mboni za Yehova , ndipo tinali ndi colinga cofanana ca kucita utumiki wa nthawi zonse . Imfa ndi Kuukitsidwa kwa Yesu — Kodi Zili ndi Tanthauzo Lotani kwa Inu ? 9 Anthu angakhale monga makina amene amangocita zimene anawakonzelatu kucita . Nkhani imeneyi idzatitsimikizila kuti Yehova nthawi zonse wakhala Mfumu ndipo idzaonetsa mmene wasonyezela ucifumu wake ku zolengedwa zake zakumwamba ndi za padziko lapansi . N’cifukwa ciani mphunzitsi wa Mau a Mulungu ayenela kumaganizila za kufunika kwa ubatizo pamene akuphunzitsa Baibo mwana wake kapena munthu wina ? Ena amaganiza kuti akamathandiza anthu osauka kapena kugwila nchito yothandiza anthu monga udokotala , unesi kapena uphunzitsi ndiye kuti akulalikila . Cofunika kwambili n’cakuti timagwila naye nchito mmene tingathele . ( Luka 5 : 29 ; Yohane 12 : 2 ) Koposa zonse , Yesu anali kupeza nthawi yopemphela , yosinkhasinkha , ndiponso yopumula . — Mateyu 14 : 23 ; Maliko 1 : 35 ; 6 : 31 , 32 . ngati titonzedwa kapena kutamandidwa mopambanitsa ? ( Sal . 91 : 1 , 2 ) M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene makonzedwe a mizinda yothaŵilako angatithandizile kutengela citsanzo cabwino ca Yehova pankhani yoonetsa cilungamo na cifundo . Iwo anayamba kuzindikila kuti nthawi zokwanila 7 zidzatha mu 1914 . ( Yesaya 45 : 18 ) Tikaganizila za malo abwino okhalamo amene Atate wathu , Yehova , anatipatsa , timaona kuti iye amatikonda kwambili . — Ŵelengani Yobu 38 : 4 , 7 ; Salimo 8 : 3 - 5 . Mngelo wanga akhala patsogolo panu . ’ ( Eks . Ponena za masinthidwe aakulu amene Ufumu wa Mulungu udzacita , Mulungu anati : “ Taonani ! E . Ngati sitisamala , tingasiye kuyamikila zinthu zabwino zimene Yehova amaticitila . N’cifukwa ciani tikutelo ? Malangizo amenewa anawathandiza kwambili . 11 : 38 - 44 . Yehova anafotokoza zimenezi pamene anati : “ Atumiki anga adzafuula mokondwa cifukwa cokhala ndi cimwemwe mumtima . ” — Yesaya 65 : 14 . DZIKOLI n’lopondeleza ndi lopanda cilungamo pa zacuma . Zinthu zina zimene zingatithandize kukhala odzilanga tekha ni kupemphela mocokela pansi pa mtima , kuŵelenga Baibo , na kusinkha - sinkha . Simone , m’bale wa zaka za m’ma 40 amene anakulila ku Italy , na mkazi wake wa zaka za m’ma 30 dzina lake Anna , amene anakulila ku New Zealand , onse anasamukila ku Myanmar . Iye anati : “ Ndimakhuzidwa mtima ndi mau a Yesu akuti : ‘ Musamade nkhawa za tsiku lotsatila , cifukwa tsiku lotsatila lidzakhala ndi zodetsa nkhawa zakenso . Iye anakamba mokweza kuti : “ Sindinaseketu ine ayi ! ” Kodi Nkhani za m’Baibulo Zimatsutsana ? Nanga unathandiza bwanji kuti Yehova akhalenso ndi gulu la alambili ake padziko lapansi ? Kodi angacite bwanji zimenezi ? Monga mmene mau okambidwa pa nthawi yoyenela angakondweletsele owamva , mphatso yopelekedwa pa nthawi yoyenela , kapena pa cocitika coyenela ingacititse woilandila kusangalala kwambili . Mogwilizana ndi Cilamulo ca Mose , Aisiraeli anafunikila kupeleka nsembe zoyenela . Kodi adzaononga dzikoli kufika pati ? ( Miy . 22 : 6 ) Jimmy anauza amai ake kuti : “ Musakabwele , muzingonditumizila mphatso . ” Ngati ndinu wacinyamata , kodi mumayesetsa kupemphelela Akristu anzanu kuti mukhale nao pa ubwenzi wolimba monga abale ndi alongo anu acikristu ? Kodi Yehova anaonetsa bwanji ulamulilo wake ku Iguputo ? Nanga zimenezo zinakhudza bwanji anthu ake osankhika ? Koma ngati ndimwe oona mtima ndipo simubisa zimene mwalakwitsa , anthu adzakudalilani . Ine ndidzakokela kwa iwe m’cigwa ca Kisoni , Sisera mkulu wa gulu lankhondo la Yabini , pamodzi ndi magaleta ake ankhondo ndi gulu lake lonse . Pamenepo ndidzam’peleka m’manja mwako . ” — Ower . Onani kuti Yesu anakamba kuti anadziŵitsa dzina la Mulungu . M’kupita kwa nthawi , Mfumu yathu inaphunzitsa anthu ake kuti akhale aphunzitsi aluso pogwilitsila nchito Sukulu ya Ulaliki . Kodi zinthu za kuthambo zimawonongeka m’kupita kwa nthawi ? Zimenezi zingapangitse kuti tibwelele m’mbuyo potumikila Mulungu . — Miyambo 13 : 12 . M’magazini anu muli umboni wosonyeza kuti Mboni za Yehova zimam’khulupilila Yesu . Poyamba , maina awo anali Abulamu ndi Sarai . Koma amadziŵika kwambili na maina amene Yehova anawapatsa . — Genesis 17 : 5 , 15 . Mpaka kumapeto kwa zaka za m’ma 1800 , madokota nthawi zambili anali kusamalila mitembo kenako n’kusamalila anthu odwala , cosasamba m’manja . 103 : 8 . Tinali kusangalala ngako na nchito yoyendela cigawo . 4 : 16 ) Dziko lonse lapansi lidzakhala paradaiso wosangalatsa kwambili , ndipo aliyense padziko adzaonetsa cikondi ca Mulungu . Iwo anali kuyenda wapansi kapena kukwela bwato , ndipo m’njila anali kukumana ndi zoopsa zosiyanasiyana . Uthenga wa Mulungu wochulidwa m’Baibulo wakhudza kwambili umoyo wathu , ndipo udzapitilizabe kukhala wamphamvu pa ife . Koma ngati Yesu anatengedwela ku kacisi m’masomphenya , ena angafunse kuti : KODI INU MUONA BWANJI ? Kodi Akristu odzozedwa okhulupilika aonetsa bwanji kuti ndi okonzeka kubwela kwa Yesu ? ( Yoh . 15 : 15 ) Komabe , kodi n’ciani cinacitika Yesu atamangidwa ? Monga mmene tionele m’nkhani zitatu zotsatila , ambili apeza kuti kuseŵenzetsa malangizo a m’Baibo kwaŵathandiza kwambili kulimbana na mavuto mu umoyo . ( Afilipi 2 : 20 ) Mbili yabwino imeneyo sinangobwela mwangozi . Pamene ndinam’funsa zimene anali kucita , anandiuza kuti , ‘ Ndikuyelekezela kukhala wacinyamata wa pa Beteli ndipo ndikufuna kuŵelenga Baibulo kwa caka cimodzi . ’ ” Koma anaona “ Mfumu ya mafumu ndi Mbuye wa ambuye , ” Mfumu ya Ufumu wa Mulungu , amene adzagonjetsa adani a Mulungu posacedwa , amene ni viŵanda na anthu oipa , ndipo adzabweletsa madalitso osatha kwa anthu . — Chivumbulutso 19 : 16 ; 21 : 3 , 4 . Mungacite ciani ngati m’banja lanu muli vuto la kusiyana zitundu ? Cifukwa ca kupanda ungwilo , mwina ena a ife timavutika kuthetsa khalidwe la tsankho limene tinali nalo poyamba . ( Yer . 17 : 9 ; Aef . Mulungu adzathetsa mavuto . Kodi Yehova anaonetsetsa bwanji kuti cilengedwe conse cikugwila nchito mogwilizana ? N’ndani maka - maka woyenela kupatsidwa ulemu ? Ndipo n’cifukwa ciani ? Ndipo kumatithandizanso kuona mmene Mulungu amayankhila mapemphelo athu . Mpaka pano nikali kutumikila monga mmishonale ku Japan . ” Cakumapeto kwa fanizo la Yesu , anamwali opusa akupempha anamwali anzelu mafuta oika m’nyali zao . Kodi Ababulo anayesa bwanji kusintha Danieli kuti agwilizane na cikhalidwe ndi cipembedzo cawo ? Yehova amathandizanso atumiki ake kupilila mavuto aakulu . M’nthawi ya atumwi , Akristu anazunzidwa ndipo cikhulupililo cao cinayesedwa . Ngakhale zinali conco , anthu ambili anakhala Akristu . ( Mac . Nkhanizi zidzatithandiza kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova Mulungu . Ngakhale kuti anthuwo sanali kutsutsa malemba mwacindunji , io anali kucititsa magaŵano . Mphepo inali kuloŵa kwambili m’mipata ya matabwa , conco tinacita kutsekamo na manyuzipepa . 6 : 1 - 4 ) Kuwonjezela pa kukopa angelowo na khalidwe la ciwelewele , mwina Satana anawakopanso mwa kuwalonjeza kuti adzakhala na mphamvu yolamulila anthu onse . Conco , mau ena a m’buku la nyimbo anasinthiwa kapena kucotsewa kuti agwilizane na mau amene ali mu Baibulo la Dziko Latsopano limene linakonzedwanso mu 2013 . Kodi panthawi ino Yehova akutiphunzitsa ciani pa nkhani ya kukhululuka ? Nanga zimenezo zidzatipindulitsa bwanji m’dziko latsopano ? O’Connor na anthu 100 acipongwe anayesa kusokoneza msonkhano wina umene m’baleyu anacititsa ku Dublin , koma omvetsela anacita zotheka pomuikila kumbuyo mlankhuliyo . Kuti timvetsetse phindu la cilango , tiyeni tikambilane za anthu aŵili amene anapatsidwako cilango na Yehova . Ndiponso , gulu la Yehova limakonza misonkhano imene imacitika m’mipingo yoposa 110,000 padziko lonse . Nanga n’ciani cidzacitikila Satana amene wabweletsa mavuto a anthu ? Coyamba , muzipempha Mulungu kuti akupatseni mzimu wake umene udzakuthandizani kukhala na cikondi . Maganizo olakwika a mwana amene tamuchula kuciyambi kwa nkhani ino , okhudza kumene kumacokela mitambo , ni nkhani yaing’ono . “ [ Tili ndi ] ciyembekezo ca moyo wosatha , comwe Mulungu amene sanganame , analonjeza kale - kale . ” — Tito 1 : 2 . Cifukwa cokhala woceleza , iye amalimbikitsa acicepele ndi atsopano m’coonadi . TSAMBA 28 • NYIMBO : 70 , 57 Yehova anapangitsa kuti kucite mabingu , mphenzi , na utsi , ndipo panamveka kulila kwamphamvu kwambili kokhala ngati kwa lipenga . ( Eks . Kumeneko , ang’ono anga anali kudya bwino . NYIMBO : 136 , 139 Tingakhale na cidziwitso ca m’Malemba , ndipo tingamapezeke pa misonkhano nthawi zonse , koma zimenezi pa zokha sizingaticititse kukhala anthu auzimu . Kodi pa Cikumbutso amagwilitsila nchito zizindikilo ziti ? Mu 1952 , Maria anaweluzidwa kuti akhale m’ndende kwa zaka 10 . Golec ) , Na . Ndiyeno , anapangitsa Hava kukhulupilila kuti safunika kumvela Mulungu mwa kukamba kuti : ‘ Mulungu akudziŵa kuti tsiku limene mudzadya cipatso ca mtengo umenewu , maso anu adzatseguka ndithu . ’ Mau a Mulungu amafotokoza kuti “ cikhulupililo mwa Mulungu ” ni “ maziko ” amene amafunika kuti munthu akhale Mkhiristu , ndi kuti apitilize kukhala Mkhiristu . 6 : 4 , 9 - 13 ) Ngakhale kuti anadziŵa kuti Yehova adzawononga anthu oipawo , iye anali wokhumudwa ndi makhalidwe awo osaopa mulungu . N’zitsanzo ziti zotionetsa kuti n’zotheka anthu opanda ungwilo kulemekeza Mulungu ndi ufulu wawo ? Inde , citani zinthu mogwilizana ndi pemphelo lacitsanzo . Tangoganizilani : Tili na mwayi wodziŵa Mfumu ya Cilengedwe Conse . Satana anati : “ Munthu angalolele kupeleka ciliconse cimene ali naco kuti apulumutse moyo wake . ” ( Sal . 133 : 1 ) Pamene Aisiraeli anali omvela Yehova , anali kukhala adongosolo ndi ogwilizana . Mtumwi Paulo anayamikila Akhristu a ku Korinto amene mokondwela ndi mowoloŵa manja anathandiza Akhristu anzawo a ku Yudeya . ( Sal . 55 : 22 ) Inde , tiyeni tikhale na cidalilo cakuti Mulungu angathe “ kucita zazikulu kwambili kuposa zonse zimene timapempha kapena kuganiza , malinga ndi mphamvu yake imene ikugwila nchito mwa ife . ” ( Aef . Kwa zaka zambili , ulamulilo umenewu wabweletsa mavuto adzaoneni kwa anthu . Iye anati : “ Mkwati anafika . ” Pomuphunzitsa , angamuuze cifukwa cake zimene wacita si zabwino . Tinaŵayewa kwambili koma tinakondwela kuona kuti asankha kuseŵenzetsa umoyo wawo kucita utumiki wa nthawi zonse . Koma sikuti utumiki umenewu ulibe mavuto . N’ciani cacititsa zimenezi ? 3 : 5 ) Cinanso , tifunika kuyesetsa kulamulila maganizo athu , ndi kupewa kukamba zinthu zosayenela . — Aef . Kodi anthu okonda miyezo ya Mulungu angapewe bwanji kusoceletsedwa ndi mabodza a Satana ? Kodi imfa inaloŵa bwanji m’banja la anthu ? Yesu anatipatsa nchito yolalikila ndi kuphunzitsa anthu uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . ( Mat . Nanga ndi zinthu ziti zimene Yehova amatiphunzitsa zimene zimaonetsa mmene amatikondela ? Yehova amateteza anthu onse amene amam’konda ndi kumumvela . Ndithudi , moyo wake unali waphindu . 10 : 40 - 42 ; 25 : 40 , 46 ; 2 Tim . Cacitatu , taganizilani ponena za kusintha kwa kamvedwe pa mfundo za coonadi kumene kwacitika posacedwapa . N’zacisoni kuti kupandukila Mulungu kunapitiliza . Kodi mumasintha mwamsanga ? Koma wakhala akutipatsa zilizonse zofunikila mu umoyo wathu . ” Nawonso ana amatengela zilizonse zimene timakamba na kucita , ndipo akaona kuti zimene timacita sizigwilizana ndi zimene timawaphunzitsa , iwo amatiuza . ” — David . A Mboni amaphunzitsa Baibulo komanso amacita zimene limaphunzitsa . ( Aroma 12 : 2 ) Kodi timayesetsa kutelo ? Si ndalama zokha zimene tingacite copeleka . Nili na nthawi yoculuka yokhala na mwamuna wanga , ndipo izi zalimbitsa kwambili mgwilizano wathu . Komabe , popeza kuti kuŵelenga Baibo n’kofunika ngako , onani pa kamutu kakuti “ Yesani Kucita Izi , ” pamene pali malangizo abwino amene angakuthandizeni kuti kuŵelenga Baibo kwanu kukhale kopindulitsa na kokondweletsa . N’zoona kuti pali mabuku ena akale . Panamvekanso mau ocokela kumwamba onena kuti : ‘ Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa , amene ndimakondwela naye . ’ ” Cifukwa ca mantha , ophunzila akuutsa Yesu ndi kufuula kuti : “ Tikufa ! ” ( Mat . Ndipo kupanduka kwawo kunacititsa kuti atalikilane ndi Yehova , ndaŵa ni ‘ woyela kwambili cakuti sangaonelele zinthu zoipa . ’ Ndipo lipoti la wofalitsa aliyense limaikidwa pamodzi ndi lipoti la padziko lonse . Zimenezi zimathandiza gulu kukonzekela pasadakhale za nchito yolalikila yamtsogolo . Mofanana ndi munthu ameneyu , caka ciliconse anthu masauzande ambili amabwela mumpingo wacikhristu , ndipo amapeza mtendele umene anali kusoŵa . Tikam’dziŵa bwino Yehova ndi kum’konda kwambili , tidzayandikila kwa iye . — Ŵelengani Salimo 25 : 14 . ( b ) Kodi malamulo amene Yehova amatipatsa amakhala otani ? Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi . . . Ngati dzila la mkazi silinalumikizane na mbeu ya mwamuna , mimba siingakhale . Poyamba Aisiraeli ayenela kuti anakondwela kwambili ndi cakudya cozizwitsa cimeneci . Ayenela anaganiza kuti anthu amenewo anali kusokoneza udindo wa Mose ndi ulamulilo wake . 15 , 16 . ( a ) Tingacite ciani kuti tipindule na “ mphatso za amuna ” mu mpingo ? Nthawi zonse ndimakhalila kudziimba mlandu ndipo ndinali kukaikila ngati Yehova angandikhululukile pa zoipa zonse zimene ndinacita . Kale sitinali kucita kulambila kwa pabanja . 3 : 1 ) Koma zingatheke cifukwa ca thandizo la Yehova . “ Mulungu ndiye Mzimu , ” conco sitingamuone . Mwacitsanzo , mvelani zimene wansembe wina amene anakhalako m’maiko osiyanasiyana anauza Mboni za Yehova . 6 : 1 - 4 . Akulu amayesetsa kupeleka thandizo lauzimu kwa amene atenga njila yolakwika ( Onani ndime 17 ) Kupatsa ni limodzi mwa makhalidwe apadela a Mlengi wathu , Yehova Mulungu . ( 1 Akor . 15 : 45 ) Mwakutelo , Yesu anacita zambili kuposa pa kubwezeletsa cabe moyo . Conco , kaya ndife odzozedwa na mzimu kapena tili na ciyembekezo codzakhala na moyo wosatha m’paradaiso , tifunika kuyamikila malangizo ouzilidwa a pa Aroma caputa 8 . Baibulo limaphunzitsa kuti kulanga kumatanthauza kuphunzitsa , kutsogolela , kuongolela , ndiponso nthawi zina kupeleka cilango . Atafika zaka 15 , anayamba kucita ciwelewele ndi amuna osiyana - siyana pofuna kuthetsa vuto lake la kusungulumwa . N’nabadwa pa 7 March , mu 1936 . Tinabadwa ana anayi m’banja lathu , ndipo ine ndine wothela . Ndiyeno mu 2000 , iye anasamukila ku Russia . ( 1 Mafumu 19 : 19 ) Covala cimeneci cinali copangidwa ndi cikopa ca nkhosa kapena mbuzi ndipo anali kucivala monga mkhanjo umene unali kuonetsa kuti anapatsidwa nchito yapadela ndi Yehova . ( Aefeso 4 : 28 ) Kunena zoona , ngati tigwila nchito mwamphamvu timapeza zosowa zathu ndi za banja lathu , ndipo tingathandizenso anthu ena ovutika . Zimene zinanicitikila mu umoyo wanga , zanithandiza kukhala woganizila ena ndi wacifundo , maka - maka kwa anthu amene akukumana na mavuto . ( Mat . 19 : 5 , 6 ) Panopa , kuposa ndi kale lonse , tiyenela ‘ kucita ciliconse cotheka kuti iye adzatipeze opanda banga , opanda cilema ndiponso tili mu mtendele . ’ — 2 Pet . 27 : 1 , 2 , 24 - 26 ) Komabe , dzina lake limapezekanso nthawi zambili m’mabuku ena a mbili zakale . Koma bwanji imwe pamwekha ? M’maiko ena , acicepele amakakamizidwa kukhala na zolinga monga kucita maphunzilo apamwamba ndi kupeza nchito ya ndalama zambili . ( Yohane 17 : 3 ) Kukamba zoona , tidzalandila madalitso osatha ngati ticita khama kuti tidziŵe Yehova Mulungu na Mwana wake , Yesu Khristu , komanso kucita zinthu zowakondweletsa . ( b ) N’ciani cimene cingatithandize kuti tizilalikila mogwila mtima ? Kuti tipambane polimbana ndi Satana sitiyenela kugonja tikayesedwa kuti ticite ciwelewele . — 1 Akor . Iwo anaona zinthu zolimbikitsa zimene akanauzako ena ‘ posimba nchito zolungama za Yehova . ’ ( Ower . Kucita izi kudzatithandiza kukapeza ufulu weni - weni . Mtumwi Paulo analimbikitsa okhulupilila anzake kupeleka “ nsembe ” zacitamando kwa Mulungu . ( Aheb . Kodi ndine womasuka nao cakuti amatha kundiuza ciliconse , ndipo angathe kundipempha thandizo ngati ayesedwa kuonelela zamalisece ? ’ Ndipo pa vesi 28 pakuti : “ Mwa njila imeneyi amuna akonde akazi ao monga matupi ao . ( Mat . 9 : 36 ) Yesu anadziŵa cifukwa cake anthuwo anali otayika ndi onyukanyuka mwauzimu . Atsogoleli awo acipembedzo anali kuwaphunzitsa mabodza na kuwapondeleza . Iye analinso kupita kunyumba ndi nyumba kupemphetsa ndalama za cipani cao . 3 Anadzipeleka Mofunitsitsa — Ku New York ( Aefeso 5 : 25 ; 6 : 4 ) Tinayamba kucitila zinthu pamodzi monga banja . Atafika , anadabwa kuona kuti magulu aŵili a asilikali angoimilila cilili m’bwalo lomenyela nkhondo monga mmene takambila poyamba paja . Ena amakhulupilila kuti Mulungu amadalitsa na kutembelela anthu ena . Ena amakhulupilila kuti Mulungu amaona anthu onse cimodzi - modzi . Ena atengela citsanzo ca Mose ndi makolo ake , mwa kusiya umoyo wabwino ndi wochuka . Ndipo nthawi zambili makolo amavutika kuteteza ana awo ku makhalidwe oipa amenewa . Philip amakumbukila kuti kwa zaka zambili , zocita zake zinali kuonetsa kuti sanali kufuna maudindo oonjezeleka mumpingo . Monga tate , Yehova anaonetsa kuti amakonda Yesu pamene anati : “ Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa , amene ndimakondwela naye . ” — Mat . Mofanana ndi Akristu a m’nthawi ya atumwi , io anali kagulu kocepa , ndipo anali kulalikila uthenga umene anthu ambili sanali kusangalala nao . 25 : 11 . Izi zili conco cifukwa onse aŵili amalakwa . ( Danieli 12 : 13 ) Yesu anauza Asaduki , atsogoleli a Ayuda amene anali kukana kuti akufa adzauka , kuti : “ Mukulakwitsa cifukwa simudziŵa Malemba kapena mphamvu ya Mulungu . ” Komabe , m’bale winayo anam’kumbutsa kuti mlongoyo watumikila Yehova mokhulupilika kwa zaka 40 ngakhale kuti akukumana ndi mavuto ambili . Cifukwa cakuti Solomo anali kunyalanyaza malamulo a Yehova , m’kupita kwa nthawi anacita macimo aakulu kwambili . Anali kuseŵenzetsa zimene anaphunzila kwa ena . Iwo afunika kumvela cenjezo , kutengela Khiristu , kudzipeleka kwa Mulungu , ndi kucilikiza abale a Khiristu pa nchito yolalikila uthenga wabwino . Nkhani yakuti “ Mafunso Ochokera kwa Owerenga ” ya mu Nsanja ya Olonda ya July 15 , 2002 , inafotokoza kuti mlongo ayenela kuvala cakumutu ngati akucititsa phunzilo la Baibulo limodzi ndi mwamuna kaya ndi wobatizidwa kapena ai . Tsopano Sauli ndi asilikali ake anapeza mphamvu . Mwacitsanzo , kwa Ayuda amene anali kufuna kuti awaonetse cizindikilo , iye anawauza kuti : “ Gwetsani kacisi uyu , ndipo ine ndidzamumanga m’masiku atatu . ” Anthu amene amakoka fodya si okhawo amene amavutika . 8 Kodi Mumam’dziŵa Yehova Monga Mmene Nowa , Danieli , na Yobu Anam’dziŵila ? Koposa zonse , anafunika mzimu woyela wa Yehova , umene ukanawathandiza kucita zinthu mogwilizana na nzelu , cifundo , na cilungamo cake . — Eks . Ganizilani mmene Hana anayewela kukumbatila mwana wake , kuseŵela naye , kum’phunzitsa , ndi kucita zinthu zina zosiyana - siyana zimene mayi wacikondi amacita ndi mwana wake wam’ng’ono akamakula . Ndi zinthu ziti zimene Yehova anakucitilani zimene mumayamikila ? ( Miy . 12 : 16 , 23 ) Mlongo wina wa ku Australia anati : “ Apongozi anga aamuna anali kutsutsa kwambili coonadi . 3 : 12 , 13 . “ Pamene pali mzimu wa Yehova , pali ufulu . ” — 2 AKOR . ( Welengani 2 Timoteyo 2 : 2 ) Komabe , mofanana ndi akulu amene tawachula m’ndime yoyamba , mungaone kuti kucita zimenezi n’kovuta . ( Mat . 6 : 10 ) Monga Mfumu yosankhidwilatu , Yesu anauza anthu amene anali kumutsutsa kuti : “ Ufumu wa Mulungu uli pakati panu . ” Tingaonetse mwa zokamba ndi zocita zathu . Apo ayi , ndiye kuti cikhulupililo cathu sicokwanila . Afilisiti anamanga msasa pakati pa mizinda iŵili imeneyi , m’mbali mwa phili limene mukuliona . ( Aroma 10 : 2 ) Conco , sitiyenela kuganiza kuti ngati munthu tamuŵelengela lemba , ndiye kuti basi adzamvetsetsa tanthauzo lake . Kale kwambili Cilamulo cisanaleke kugwila nchito , Yehova anakambilatu kupyolela mwa mneneli wake Yeremiya kuti , adzacita “ pangano latsopano ” ndi mtundu wa Isiraeli . 17 , 18 . Koma Yesu anawalangiza kuti ayenela kupemphela moona mtima osati ndi colinga cakuti ena awatamande . Sitiyenela kufulumila kupeleka uphungu kwa ena . Gulu la Yehova latipatsa zida zambili zimene zingatithandize kukhala na phunzilo laumwini lopindulitsa . Ngakhale anthu amene amatitsutsa ndi kukana uthenga wathu tiyenela kuwathandiza akafuna thandizo . Mkaziyu anaonetsa kuika cidalilo conse mwa Yehova , podziŵa kuti akaika zinthu zauzimu patsogolo , Mulungu adzasamalila zosoŵa zake zakuthupi . Koma yoposa zonse , n’kutangwanika m’nchito yolalikila , podziŵanso kuti imalimbitsanso ciyembekedzo cathu . Kuukitsidwa kwa Yesu kunawakhudza kwambili ophunzila ake . Kodi anangosintha mwadzidzidzi cifukwa coganiza kuti moyo wosatha pano padziko lapansi sudzakhala wosangalatsa ? Nkhani yokhudza mfumu inapangitsa mtima wa wamasalimo kuŵila cifukwa ca cisangalalo ndipo lilime lake linakhala ngati “ colembela ca wokopela malemba waluso . ” Sitiyenela kukonda kwambili dziko lathu kapena mtundu wathu n’kumaona kuti maiko ena ndi mitundu ina si zabwino kwenikweni . Pamene mapeto a dziko loipali akuyandikila , n’zodziŵikilatu kuti mavuto aziculukila - culukila . 2 : 16 , 17 ) Njoka inamuuza kuti : “ Kufa simudzafa ayi . Atavala zovalazo , Davide anafuna kuyenda , koma anaona kuti sangakwanitse kuyenda nazo . Pokamba za cilengedwe , mtumwi Paulo analemba kuti : “ Makhalidwe a Mulungu osaoneka ndi maso akuonekela bwino . Conco , m’malo mom’kaikila , ndinayang’ana pa makhalidwe ake abwino kuti ndim’limbikitse . ” Kuonjezela pamenepo , tinalandila zovala zamphepo , nsapato , zola [ zikwama ] , ndi zovala zamkati . ” Tsiku lina pamene iye ndi atate wake anali kucokela mu ulaliki wakumunda , anapitila njila yodutsa pa mtsinje wina wake . akumveka ( vesi 6 ) ndi kubwela kapena kufika kwa mkwati ( vesi 10 ) . Sara anakonza mkate umenewu mofulumila ndipo mwina anauphikila pamiyala yotentha . — 1 Mafumu 19 : 6 . Acikulile ena anali ndi umoyo wa wofuwofu akalibe kukalamba , ndipo angafunike kusintha kuti akhale ndi umoyo wosalila zambili ndi kukhutila ndi zocepa zimene ali nazo . Njila ina imene ingatithandize kuti tidziŵane bwino na anthu ocokela ku maiko ena , ndi kuŵaitanila ku cakudya kunyumba kwathu . Odzozedwa amene amatsiliza moyo wao wa padziko lapansi mokhulupilika , amaukitsidwa kupita kumwamba ndi kupatsidwa moyo wosafa . ( 1 Akor . Zokamba zathu . Kodi tingaphunzilepo ciani pa zimene zinacitikila Yobu ? Koma amene amagwila nchito yoculuka mwa kufuna kwake , amakhala womasuka cifukwa amacita kusankha yekha kugwila nchitoyo . Rico anaganiza kuti akakula m’pamene angatumikile Yehova . Patapita nthawi yocepa , nduna ya zamaphunzilo ya m’dzikolo inapita ku tauni kumene kuli sukuluyi , ndipo inakambilana ndi ana a sukulu ena a Mboni . 2 : 17 ) Conco , ni bwino kumapatsa moni anthu ena , mosasamala kanthu za mtundu wawo , cikhalidwe , kapena kumene anakulila . Iwo anati : “ Kuganizila mozama zinthu zimenezi kwaticititsa kuona kuti luso la zopangapanga laononga cikhalidwe ca anthu . ” Kwa zaka 12 , mayiyo anali kukhala mwamanyazi . ( Maliko 14 : 34 - 38 ; Luka 22 : 24 - 27 ) Iye sanabwezele ngakhale kuti anacitilidwa zinthu mopanda cilungamo . — 1 Pet . Davide anali paubwenzi wabwino ndi Yehova . Conco anapempha Yehova kuti amutonthoze ndi kumucilikiza pamene anali kudwala . Iye anati : “ Ine na mkazi wanga timacita kulambila kwa pabanja pamodzi ndi ana athu m’Cifulenci . Zoonadi , kukhulupilila magazi okhetsedwa a Yesu kumatsegula khomo kuti macimo athu akhululukidwe , komanso kuti tikapeze moyo wosatha . Pokhala Mkristu wodziŵa zambili , muli ndi mwai umene ena alibe . Mkristu wofikapo amafufuza mfundo za m’Baibulo zimene zingam’thandize kudziŵa cabwino ndi coipa Anacita izi maulendo aŵili . ( Mateyu 14 : 17 - 20 ; 15 : 34 - 37 ) Koma pamene anali ndi njala m’cipululu , Mdyelekezi anamuuza kuti asandutse miyala kukhala mkate , koma iye anakana . Komiti Yoona za Atumiki a pa Beteli Mwacitsanzo , m’bale Brandon anacita upainiya kwa zaka 9 m’gawo limene anthu analibe cidwi na uthenga wabwino . Ndikulimbitsa . ” ( Yesaya 26 : 10 , 11 ; 3 Yohane 11 ) M’nthawi ya mtumwi Paulo , ena analinso ndi maganizo amenewo . Kuonjezela pa mavuto amenewa , “ m’masiku otsiliza ” ano anthu ndi odzikonda ndipo salemekeza Mulungu . Makhalidwe amenewa angaononge cikwati . Iye anafunika kulimba mtima kuti acotse Maaka pa udindo wokhala “ mayi wa mfumu ” m’dziko lake . Kuvutitsaku sikunali kwa maseŵela cabe . Kwa zaka 6 , ndakhala m’banja lacimwemwe ndi mwamuna wanga Jonathan , amene amaopa Mulungu . Nthawi zina , inu kapena munthu wina , akhoza kucitilidwa zinthu zopanda cilungamo , kapena kuona kuti zinthu zina sizinacitike mwacilungamo mumpingo . Zikondwelelo zimenezi ndi Pasika , Pentekosite , ndi Cikondwelelo ca Misasa . 2 : 16 , 17 , 23 . 5 : 8 ) Iwo afunika kugwila nchito mwakhama kuti akwanilitse udindo umenewu . Mdyelekezi angakondwele kwambili ngati tingagonje . Ndine wokondwa kuti mkazi wanga wokondedwa wandicilikiza kwambili kwa zaka zonsezi . M’malomwake , amakhala odzicepetsa ndipo amadziŵa kuti Yehova yekha ndiye amaitana anthu kuti akapite kumwamba . Nkhondo Imene Inasintha Zinthu Padziko Kodi Mulungu adzacita ciani Satana akadzafuna kuononga anthu ake ? Ndithudi , Yehova amadalitsa nchito yolalikila imene akazi acikristu amacita , ndipo amawathandiza pa nthawi yovuta . “ Ine ndidzalemekeza malo oikapo mapazi anga . ” — YES . Yehova anadalitsa kwambili Louis na Perrine cifukwa ca kupilila kwawo . Agibeoni anali osiyana kwambili ndi anthu amene anali kukhala nao pafupi . Muzilimbikitsana Atafika ku Isiraeli , anaona kuti zinthu tsopano zinali zitasintha . Ndipo cifukwa ca ndeu , pafupifupi wikendi iliyonse ndinali kukhomeledwa ku polisi kapena kugonekedwa m’cipatala cacikulu kuti andisoke mabala a zilonda . ( Machitidwe 25 : 11 ) Ngakhale kuti Baibulo limanena kuti Satana ndiye akutsogolela maboma onse a anthu , silikamba kuti iye amatsogolela wolamulila wa boma aliyense payekha . N’cifukwa ciani analiuza kuti lisacoke ? Ngakhale kuti anthu ambili anali kulambila milungu yonama pambuyo pa Cigumula , anthu ena okhulupilika anapitilizabe kulambila Yehova . Akristu okalamba sangadziŵe mmene citsanzo cao cimalimbikitsila ena . N’ciani cinathandiza Abulahamu kukhala ndi cikhulupililo camphamvu ? Mkazi wina wa ku Germany amene ali pa banja anati : “ Mnzako wa mu cikwati amavutika mtima ngati ukana kum’lankhula . ” Kodi acinyamata angacite ciani kuti athandize mpingo kukhala wogwilizana ? Gulaye imapezeka m’zolemba za Aiguputo ndi Asuri za m’nthawi za m’Baibulo . A Daka : Inde . ( Mika 6 : 8 ) Iwo afunikanso kukumbukila kuti “ nthawi yatsoka ndi zinthu zosayembekezeleka ” zingawalepheletse kusamalila maudindo monga mmene anali kucitila poyamba . ( Mlal . Popeza kuti uthenga womwe uli m’fanizo la Yesu umakhudza otsatila ake odzozedwa , kodi tinganene kuti a “ nkhosa zina ” sangapindule ndi fanizo limeneli ? ( Yoh . Baibo imayankhanso mafunso monga akuti : Kodi ufulu wosankha zocita umenewu tiyenela kuuseŵenzetsa bwanji ? NYIMBO : 81 , 134 Pamene tikambilana mfundo zimenezi , tingacite bwino kuganizila mmene zimakhudzila ubwenzi wathu ndi Mulungu ndi zimene tingacite kuti tilemekeze Atate wathu . Malinga ndi mmene zinthu zilili kwanuko , mungapeleke zopeleka zanu m’njila izi : Kodi makolo angaphunzile ciani kwa Samueli ? 3 : 9 ) Tingatsimikize bwanji kuti Yehova amayamikila zimene timacita pomutukila mokhulupilika ? Odzozedwa onse akadzapita kumwamba , adzakonzekela komaliza ukwati wa Mwanawankhosa . ( Chiv . 2,671 Katswili wina wacipembedzo dzina lake Augustine , anafotokoza mwatsatanetsatane za nkhani ya Yesu imene timaŵelenga yakuti anadyetsa amuna pafupifupi 5,000 ndi mikate isanu ya balele komanso nsomba ziŵili . TIKUKHALA m’nthawi yovuta kwambili m’mbili yonse ya anthu . Zina mwa nyumbazo zinali na zipinda zopitilila 12 , akasupe a madzi abwino , mabafa na zimbudzi zamkati . Kodi ndinu citsanzo cabwino ku sukulu ? Lemba la 2 Mbiri 16 : 9 limandilimbikitsa . Limati : ‘ Maso a Yehova akuyendayenda padziko lonse lapansi kuti aonetse mphamvu zake kwa anthu amene mtima wao uli wathunthu kwa iye . ’ ” ( Aroma 6 : 16 ) Ngati cilakolako ca fodya cimalamulila maganizo ndi zocita za munthu , iye amakhala kapolo wa fodya . Tinasangalala kuona zabwino zimene zimatulukapo ngati ‘ tipitiliza kugonjetsa coipa mwa kucita cabwino . ’ — Aroma 12 : 21 . Kucita zimenezi kungapeleke cithunzi colakwika . Kodi n’lamtengo wapatali motani ? Zili conco cifukwa cikwati n’copatulika . Yesu atabweleza zimene Mulungu anakamba kuti mwamuna adzasiya makolo ake n’kukagwililizana na mkazi wake , anati : “ Cimene Mulungu wacimanga pamodzi , munthu asacilekanitse . ” ( Mat . 19 : 3 - 6 ; Gen . ATUMWI a Yesu anaimilila pa Phili la Maolivi , kuyang’ana kumwamba . Nanga n’cifukwa ciani anali kukamba conco ? ( b ) Tingacite ciani kuti tidziŵe bwino “ maganizo a Khristu ” ? “ MUNTHU AKAFA , KODI ANGAKHALENSO NDI MOYO ? ” Ngakhale kuti timasangalala kugona tulo twabwino , palibe amene angafune kugona osadzukanso . Kodi zimenezi n’zoona ? Iwo anali kukhala mumzinda wolemela wa Uri , umene unali ndi akatswili ambili a zopanga - panga ndi amalonda . Makolo angacite bwino kutengela citsanzo ca makolo a Danieli . Popeza n’nakhala nekha , ofesi ya nthambi inanitumizanso ku Hemsworth kuti nikatumikile monga mpainiya wapadela . Paulo ataimilila pamaso pa anthu amene anali kuphunzitsa nzelu za anthu , iye molimba mtima anaikila kumbuyo ulamulilo wa Yehova , ‘ Mulungu amene anapanga dzikoli ndi zinthu zonse zili mmenemo , amene ndi Ambuye wakumwamba ndi dziko . ’ Angakambe mabodza monga akuti : “ Musawamvele atsogoleli anu , angokunamizani , ” kapena kuti “ Samalani , adzakuphetsani . ” Koma ine sin’namasulidwe . Umboni umene Petulo anapeleka , unathandiza kwambili bungwe lolamulila la m’zaka 100 zoyambilila kupanga cosankha pankhaniyi . ( Maliko 7 : 9 - 13 ) Conco , tingakambe motsimikiza kuti otsatila oona a Yesu akhulupilila zimene Baibulo imakamba . Komanso wina anati : “ Citsanzo cawo cimanikondweletsa . ” Conco , buku la Mateyu limakamba kwambili za maganizo a Yosefe na zimene anacita . Koma la Luka limafotokoza kwambili za maganizo a Mariya na zimene zinam’citikila . Nanga abale ena masiku ano apilila bwanji cizunzo cacindunji ? Molimba mtima Paulo anapilila masautso acindunji , ndipo anati : “ Moyo wanga sindikuuona ngati wofunika kapena wamtengo wapatali kwa ine ai . Mwamacenjela , Satana anaonetsa kuti Yehova sanali kufuna kuti iwo adye cipatsoco kuopela kuti angatseguke mutu . Koma ngati tingayambe kulambila munthu kapena cinthu cina ciliconse , ndiye kuti dzina lathu lingacotsedwe m’buku la moyo lophiphilitsila la Yehova . — Eks . Monga Mphunzitsi Waluso , Yesu anapatsa otsatila ake malangizo omveka bwino a zimene anayenela kucita . Malangizo amenewa ali m’Baibo . Khalani woceleza Ulamulilo wa anthu udzatha ndipo ulamulilo wa Ufumu wa Mulungu udzayamba . 32 : 33 ; Sal . Ndinali kuganiza kuti tidzayamba kuthela nthawi yaitali kuŵelenga ndi kuphunzila Baibulo . Nikapita ku mizinda ina , nthawi zonse nimayetsetsa kulalikilako anthu ogontha . Kodi kuuka kwa Yesu kumatsimikizila ciani ? Kuti tipeze yankho , tifunika kuganizila za dziko la Iguputo wakale . ( Aroma 12 : 3 ) Tonsefe sitifuna kupangitsa abale a Kristu odzozedwa kucita colakwa cacikulu ngati cimeneci . — Luka 17 : 2 . Ndithudi , kucita zinthu mwaulemu ndi anthu ena kumabweletsa madalitso , kuphatikizapo mtendele . ( Yes . 30 : 21 ) Tinganene kuti Yesu nayenso amatiuza mau a Yehova potsogolela mpingo kupyolela mwa “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” ( Mat . Masiku ano , nkhani zimafalikila mwamsanga , kaya nkhaniyo ndi yoona kapena ai , yothandiza kapena yacabecabe , yabwino kapena yoipa . Koma mwina tingadzifunse kuti , ‘ Kodi Yehova anakhala bwanji mfumu panthawiyo popeza kuti iye ndi Mfumu yamuyaya ? ’ Mwacitsanzo , madokota amadalila dongosolo la cipangidwe ca thupi la munthu kuti agwile bwino nchito yawo . Mlongo wina pofotokoza zifukwa zimene anali kuletsela mwana wake kubatizika , anati , “ N’zocititsa manyazi kufotokoza , koma cifukwa cacikulu n’cakuti n’nali kudela nkhawa kuti angadzacotsedwe . ” Nanga aphunzila ciani potumikila ku maikowo ? Kuti tiyankhe funso limeneli coyamba tifunse kuti , Kodi moyo unayamba bwanji ? Mwacitsanzo , wacicepele angaone kuti mphatso yabwino koposa ni cipangizo camakono cimene cangotuluka kumene . ( 2 Akor . 3 : 17 ) Timaiyamikila ngako mphatso imeneyi cifukwa imatilola kupanga zosankha zoonetsa kuti Yehova timam’kondadi . Komabe , io anali kudela nkhawa mmene angalele Jacob , mwana wao wazaka 11 . Monga mlendo , kwa mawiki angapo oyambilila , mungakhale okondwa kudziŵana na anthu amene kale simunali kuwadziŵa . Ndimakonda kwambili Yehova monga mmene ndinali kumukondela poyamba . Koma pali anthu enanso amene ndimawakonda . Patapita nthawi , Elisa anabwelela ku mtsinje wa Yorodano ndipo anatenga covala cauneneli ca Eliya n’kumenya madzi a mtsinjewo , n’kunena kuti : “ Ali kuti Yehova Mulungu wa Eliya ? ” Kupitila mwa Mose , iye anawalamula kuti : “ Usadzacite nao mgwilizano wa ukwati . Nayenso Antonio atadwala , anamasulidwa . Maphunzilo amenewo anali kucitikila pa nyumba ina yaikulu yocedwa White Lodge , pafupi ndi mzinda wa London . Malinga ndi umboni wa anthu amene analipo pa nthawiyo , ambili anaphunzila coonadi mwa njila imeneyi . Pamene nchito ya Ufumu inali kukula , malo oseŵenzela pa Beteli anacepa . Nchitoyo inali yomanga kacisi ku Yerusalemu . Kodi mungapindule bwanji ndi cikondi ca Mulungu ? Pamene Yesu anali padziko lapansi , anathandiza ophunzila ake kuona kufunika kwa Ufumu wa Mulungu . Mudziŵeni bwino Yehova ndi cifunilo cake , ndipo muyandikileni kwambili . Conco kupanga zosankha zabwino n’kofunika kwambili . — Ŵelengani Aroma 14 : 19 ; Agalatiya 6 : 7 . Tingaonetse bwanji kuti timayamikila Mau a Yehova ? Anthu amene amadwala akamva fungo la pelefyumu amavutika kwambili . Cikondi ca pakati pa mwamuna ndi mkazi ( eʹros ) cimakometsa cikwati , ndipo cikondi ca pacibale ( stor·geʹ ) cimafunika pamene m’banja mwakhala ana . Muziona zimenezi kuti ndi malonjezo a Mulungu . N’zoona kuti kungaoneke kukhala kothandiza zinthu zafika povuta kwambili . Koma kaŵili - kaŵili , kupatukana kumangoitananso mavuto ena . Pamene iwo anali kukambilana , ine n’nali kumvetsela mwacidwi . Pangano latsopano ndi logwilizana ndi Ufumu mwanjila yakuti limapanga mtundu woyela , umene uli ndi mwai wodzakhala mafumu ndi ansembe mu Ufumu wakumwamba . 4 : 26 , 31 ) Malinga ndi pangano la Abulahamu , mbeu ya mkazi idzabweletsa madalitso pa mtundu wa anthu . Ndipo sicikhala covuta kwa iye kucititsa khungu maganizo a anthu otelo . ( 2 Akor . 16 : 13 , 14 ) Kodi mumzinda wa Filipi munalibe amuna aciyuda okwana 10 , ciŵelengelo comwe cinali cofunikila kuti mumangidwe sunagoge ? Pangani ndandanda yoloŵela mu ulaliki mlungu uliwonse , ndipo yesetsani kuitsatila . Pa nthawiyo tinali tikalibe kudziŵa Ciswahili , ndipo nayenso sanali kudziŵa Cizungu . Timadziŵa kuti Yehova amasankha ndi kukoka anthu oyenelela . Caka cina , ulendo wa Maria wodzaniona unali wapadela kwambili cifukwa anabwela ndi ana athu aŵili . Cakumapeto kwa zaka za m’ma 1960 , ndili pa sukulu ya sekondale , ndinaloŵa m’kagulu kandale kochedwa Black Panthers kamene kanali kudziŵika kuti kanali kumenyela ufulu wa nzika za dziko . Iye anati : “ Pemphelo , kuphunzila Baibo , ndi kusinkhasinkha zimene n’naphunzila , zinanithandiza kudziŵa bwino makhalidwe a Mulungu cakuti n’nayamba kukonda kwambili Yehova kuposa kutamba zamalisece . ” Pamene ‘ tikuyesetsa mwakhama ’ kukulitsa makhalidwe abwino monga kudziletsa , kupilila , ndi kukonda abale , tidzapitabe patsogolo monga anthu auzimu . Nafenso Akhristu tiyenela kudzifufuza kuti tione ngati timaikadi nchito pa malo oyenelela . — w17.05 , peji 22 - 23 . Conco , n’nangoganiza zocokapo . Anafe tinali mamembala a chalichi ca amai athu ca evangelical . ( Ŵelengani Akolose 3 : 5 - 10 . ) M’maiko ena , hafu ya vikwati vonse vimaesila . Pambuyo pakuti ayankhidwa ndi nthambi ya ku Ghana , anayenda kumeneko kuti akatumikileko miyezi iŵili cabe . ya February 8 , 1994 ; February 8 , 1997 ; June 8 , 2000 ; ndi ya February 8 , 2001 . ( Genesis 41 : 42 ; Yoswa 2 : 6 ) Aisiraeli a m’nthawi za Baibulo ayenela kuti sanali kulima thonje , koma Malemba amakamba kuti thonje anali kugwilitsidwa nchito ku Perisiya . 15 : 32 ) Mzimu umenewu ni wofala m’madela ambili padzikoli . Mofanana ndi Akristu oyambilila , odzozedwa amene ndi “ ana a Ufumu , ” anali kudzakhala Mboni za Yehova . Yehova amakufunilani zabwino . Conco , m’malo mowauza za ciukililo pa nthawi imeneyo , abale anangowatonthoza ndi kuwafotokozela cifukwa cake anthu abwino naonso amavutika . Pamene Carin analimbikila kuti adzalela yekha mwana wake , acibale ndi mwamuna wake anamuseka ndi kumunena kuti wafuntha . Kodi zimenezi sizikukuthandizani inuyo acinyamata kuona kuti mufunika kucita zinthu mogwilizana ndi gulu la Yehova ? Munthu wina amene anavutika kwambili ni Steve . Ali paulendo umenewu anapeza dziko la Florida , U.S.A . , ndipo anamwalila patapita zaka zocepa atamenyana ndi mbadwa za ku America . Nthawi zonse tizicita zopeleka za nchito ya padziko lonse , podziŵa kuti ndalama zimenezi zimagwilitsidwa nchito mwanzelu . — 1 Yoh . 3 : 17 . Kukhala wosamala ndi zimene timakamba zokhudza ena kudzatithandiza kukhalabe pa ubwenzi ndi Yehova . Kumene tatenga mfundo izi : Pa webusaiti yochedwa Mayo Clinic ndi Johns Hopkins Medicine komanso m’buku lakuti , Social Psychiatry and Psychiatric Epidemiology . Daniel anati : “ Tinali na umoyo umene anthu m’dzikoli amaona kuti ndiwo umoyo wabwino ngako . Pa Yohane 12 : 42 pamati , “ ambili , ngakhalenso olamulila anamukhulupilila [ Yesu ] , koma cifukwa ca Afarisi sanavomeleze poyela , poopa kuti angawacotse musunagoge . ” Munthu wina amene anali na vuto laconco ndi Nikodemo . Mukamacita zimenezi , mudzapeza cimwemwe coculuka pa nchito yolalikila . Komabe , Aroma caputa 8 ni yofunikanso kwa aja odzakhala padziko lapansi , ndaŵa nawonso Mulungu amawaona kukhala olungama . Tingasangalale kuwaona atatengelanso zitsanzo zabwino . Kulimba mtima kunathandiza Yosefe , Rahabi , Yesu , ndi atumwi kucita zinthu zoyenela . Kodi mukuyendela limodzi ndi gulu limeneli ? Tikatelo , tidzakhala paubwenzi wolimba kwambili ndi Yehova . Kumasuka kwa Aisiraeli mu ukapolo wankhanza ku Iguputo kunali kwapadela , cifukwa Mulungu analoŵelelapo . 9 : 20 - 23 . ( Luka 24 : 27 , 32 ) Pambuyo pake ophunzilawo anati : “ Kodi si paja mitima yathu inali kunthunthumila pamene anali . . . kutifotokozela Malemba momveka bwino ? ” — Luka 24 : 27 , 32 . Gavin anatsitsimulidwa ndi makambilano amenewo , ndipo anayamba kuphunzila Baibulo . 28 : 20 ) Tili ndi cidalilo cakuti , kaya adani athu acite zotani sangatiletse kulalikila . Conco , Paulo anafunika kuwakumbutsa kuti Akhiristu ali ndi Mulungu mmodzi , Yehova . — Ŵelengani 1 Akorinto 8 : 5 , 6 . Pamenepa , Asamariya anali kufuna kuti Malemba agwilizane ndi nchito yawo yomanga kacisi ku “ Gerizimu ” kapena kuti pa Phili la Gerizimu . ‘ Kucokela kwa iye , thupi lonselo . . . ndi lolumikizika bwino ndi logwilizana . ’ ​ — AEFESO 4 : 16 . Mfundo yoyamba ndi yakuti Yesu anapatsa ophunzila ake odzozedwa udindo wofunika kwambili wolalikila ndi kuphunzitsa anthu kuti akhale ophunzila . Udindowu uli ngati cuma camtengo wapatali . N’cifukwa ciani ulamulilo wa Mulungu ndiwo wabwino koposa ? Baibulo limatiuza kuti Mlengi ali ndi ‘ mphamvu zoculuka ndi zoopsa . ’ Mu 1957 , iwo anabwela m’dziko la Puerto Rico . Yehova anasintha maganizo ataona kuti Anineve alapa ndi kusiya njila zawo zoipa . Komabe , cikondi cozikidwa pa mfundo za m’Baibulo ( a·gaʹpe ) , n’cimene maka - maka cimathandiza kuti cikwati cikhale copambana . Ni mfundo iti ya m’Malemba imene inam’thandiza ? Nimasangalala ndi utumiki wa pa Beteli cifukwa umapeleka mwayi wotumikila ena . Ngati Mkhiristu akuloŵela njila yolakwika popanda iye kuzindikila , amuna ofikapo ayenela kum’thandiza ndi mzimu wofatsa . — Agal . ( Chivumbulutso 6 : 8 ) Mlili waukulu woyamba m’zaka za m’ma 1900 unali fuluwenza ya ku Spain . Mofanana ndi munthuyo , Yesu asanapite kumwamba , anali ndi cinthu ca mtengo wapatali . Mwacitsanzo , Bok - im wa ku South Korea wa zaka 69 ali ndi maganizo oyenela pa nkhani ya zovala . Iye anavomeleza kuti anacita zolakwa pamene ‘ anali mnyamata . ’ ( Sal . 65 : 2 ) “ Tate wacifundo cacikulu ndi Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , ” adzapeleka mosaumila thandizo lakuthupi ndi lauzimu limene tingafunikile . Angacite zimenezo ngakhale kupitila mwa Akhiristu anzathu . Olo zinali conco , mfumuyo na asilikali ake “ anamvela mau a Yehova n’kubwelela kwawo malinga ndi mau a Yehova . ” Iwo anali kufunika kumulandila bwino . Komanso bwanji ngati mwapeza njila zina zimene zingakuthandizeni kuti muzisangalala poiŵelenga ? 17 , 18 . ( a ) Ndi zitsanzo ziti za m’Baibulo za anthu amene anakonza zinthu zoonongeka pa malo olambilila ? Ngati takhala na cizoloŵezi colimbikitsa ena , nawonso azitilimbikitsa . — Luka 6 : 38 . Mwacitsanzo , kafuku - fuku aonetsa kuti kaŵili - kaŵili acicepele amapewa kugonana asanaloŵe m’cikwati ngati aphunzitsidwa momveka bwino kuipa kwa khalidwe limeneli . Ndiyeno , ana a Ufumu adzasonkhanitsidwa pamodzi . Mose anauza Aisiraeli kuti : “ Ndaika moyo ndi imfa , dalitso ndi tembelelo pamaso panu . Kumwamba ndi dziko lapansi ndi mboni pa zocita zanu . Tumapepala tumenetu tumaonetsanso kabuku kakuti Uthenga Wabwino Wocokela Kwa Mulungu , ndi kusonyeza phunzilo logwilizana ndi nkhani ya m’kapepala kalikonse . ( Mat . 16 : 24 ) Monga mmene Yesu analonjezela , tidzakhala na ufulu weni - weni pamene tidzalandila madalitso onse a nsembe ya dipo lake . Komabe , ife Mboni za Yehova timapewa kupeleka ulemu wapadela kwa atsogoleli acipembedzo , ngakhale kuti iwo angafune kuti ticite zimenezo . M’bale Russell anayendela dziko la Ireland maulendo 7 . Ndimalikonda cifukwa palibe buku lina loposa Baibulo . ( Yohane 14 : 31 ) Yehova akanakhala kuti anali kucita zinthu mwankhanza , Yesu sakanakamba zimenezi . Utumiki woyamba , anatituma ku ofesi ya nthambi ya ku Malawi kumene ana athu ndi amuna awo anali kutumikila . Malamulo anu amandicititsa kukhala wanzelu kuposa adani anga , cifukwa ndi anga mpaka kalekale . Solomo anali mfumu imene inalandila zambili kucokela kwa atate ake , Davide . Iye akuyamikila makolo ake cifukwa com’thandiza kudziŵa kuti zinthu zimenezi n’zofunika kwambili . Kodi aja amene amakonda kufunsila kwa olosela zam’tsogolo masiku ano , iwo zinthu zimawayendela bwino ? Yehova anatsimikizila Abulahamu kuti Hagara na mwana wake adzawasamalila . 5 : 41 ) Mwacionekele , atumwiwo sanali kusangalala cifukwa cokwapulidwa . N’zokondweletsa ngako kuona mmene Yehova akuthamangitsila nchito yake . Kodi nafenso sitiyenela kucita khama kubwelelako kwa anthu acidwi ndi kuphunzila nawo Baibulo ? Iwo ananditsimikizila kuti Yehova adzandithandiza . Iwo amalonjeza kuti adzakondana , kusamalilana , ndi kulemekezana ‘ pa nthawi yonse imene aŵiliwo adzakhala ndi moyo padziko lapansi , mogwilizana ndi zimene Mulungu anakonza pa nkhani ya cikwati . ’ Baibulo limayelekezela mamvekedwe odziŵika bwino a lipenga ndi mau osavuta kumva . Ni zinthu zopanda cilungamo ziti zimene zinacitikila m’bale wina mumpingo ? Nanga ni makhalidwe ati amene anamuthandiza kuti asakhumudwe ? Tifunikanso kukhulupilila Mau a Yehova , kudalila malangizo ake ouzilidwa , ndi kukhulupilila kuti kacitidwe kake ka zinthu ndiye koyenela . Kodi kufunsa mafunso kungatithandize bwanji kudziŵa cifukwa cake womvela wathu amakhulupilila nkhani inayake ? Iye anadziŵa kuti mwamuna wake anali na mbali yofunika kwambili pokwanilitsa colinga ca Yehova codzatulutsa mbeu komanso mtundu wodalitsidwa . Iwo adzafuula kuti : “ Ambuye , ambuye , titsegulileni ! ” Dzina la “ Wam’mwambamwamba pa dziko lonse lapansi ” — Salimo 83 : 18 , Buku Lopatulika . Tingacite bwino kudzifunsa kuti : ‘ Kodi nimakonda kuceleza mabwenzi anga okha - okha , anthu ochuka , ndi aja amene nimaona kuti nthawi ina adzanicitilako zabwino monga zimene nawacitila ? Conco n’nayamba kukhulupilila kuti n’zotheka ine kudzakhala na moyo wamuyaya m’paradaiso padziko lapansi . — Salimo 37 : 29 . Iye anati : “ Conco pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzila anga . ” ( Mat . Mtumwi Paulo anafotokoza cifukwa cake kukhulupilila kuti akufa adzauka n’kofunika kwambili pa cikhulupililo cathu . Iye anati : “ Cifukwa ngati akufa sadzauka , ndiye kuti Khristu nayenso sanauke . ” Kaya yankho lake ndi lotani , timamuonetsa mkati mwa kapepalako ndi kumusonyeza zimene Baibulo limanena . Matauni amenewo ni Hlybokyy Potik , Serednye Vodyane , na Nyzhnya Apsha . Ganizilani citsanzo ici : Ngati mwanyula mtengo pamalo ena kuti mukauwokele pena , umayamba wakwinyilila . ( Yohane 11 : 36 ) Sikuti timangoyelekezela mwaciphamaso kuti ndife abale ndi alongo . Kodi aliyense payekha afunika kutsimikizila za ciani ? 5 : 14 ; Aef . Tikamagwila mwacangu nchito yopanga ophunzila , timalimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova . Kodi mkulu angacite bwanji zimenezi ? ( Salimo 36 : 9 ) Iye analankhula ndi anthu ndipo anatiuza zinthu zokhudza iye . — Ŵelengani Yesaya 45 : 18 . Pamene anali kukambitsilana , mwamuna wake anakamba kuti amakhulupilila Utatu . Ngati tagwela m’ciyeso cimeneci , sitingaimbe mlandu Satana . Anthu onse amene amamanga banja ndi opanda ungwilo . Mulungu anawauza kuti : “ Mubelekane , muculuke , mudzaze dziko lapansi . ” Yesu sanali kungomvela ena cifundo , koma cifundo cinali kum’limbikitsa kuthandiza ena . — Mat . N’ndani afunika kulimbikitsidwa masiku ano ? Iye amatithandiza mmene tingakhalile pamtendele ndi ena , ndipo amatiphunzitsa mmene tingaphunzitsile ena za iye . ( Yesaya 48 : 17 , 18 ) Zoonadi , timakhala na umoyo waphindu kwambili pamene tilambila Wolamulila wa cilengedwe conse na kucita zinthu zom’kondweletsa . Kulibe munthu wanzelu amene angaifune . Phunzilani zambili zokhudza Yesu Kristu ndi kumukhulupilila . Koma anali na cikhululupililo cakuti Yehova adzamuukitsa Isaki . ( 1 Akor . 8 : 1 ) Pacifukwa cimeneci , pitilizani kukhala wodzicepetsa ndi kulimbitsa cikhulupililo canu . Nditafika kunyumba ndinacitadi zimenezo ndipo kwa masiku angapo ndinali kusinkha - sinkha ndi kupemphela . Kodi imeneyo siinali nthawi yosangalatsa kwa inu ? Nafenso tingaonetse Yehova kuti timam’konda mwa kum’patsa ‘ zinthu zathu zamtengo wapatali . ’ Koma kucita zimenezi kumabweletsa mavuto . 2 : 5 ) Mosakaikila , uthenga wa Nowa unaphatikizapo kuuza anthu kuti alape ndi kuwacenjeza za cionongeko cimene cinali kubwela . Koma anthuwo sanamvele . Mike ndi banja lake amadalila Yehova . Mwa kukhala wokhulupilika , Yesu anaonetsa kuti n’zotheka munthu wangwilo kusungabe miyezo yolungama ya Mulungu . Oyang’anila dela ndi akulu amakumbukila Bungwe Lolamulila mwa kutsatila mosamalitsa malangizo amene amapatsidwa . Iye analoŵa pakati pa khamu pamene panali Yesu ndi kugwila covala cake cakunja . ( Lev . Ambili a io amatengedwa kundende zimene amagwilitsa nchito ya kalavulagaga . Yehova wapatsa Solomo , mwana wa Davide , nchito yapadela yomanga kacisi kuti azilambililamo Mulungu woona . 6 : 18 . Umboni wina ni wakuti Mulungu amatisamalila ndi kutiphunzitsa mmene tingakhalile na umoyo wabwino . Ngakhale kuti pamakhala zotulukapo zabwino , kulimba mtima kwa atumiki a Mulungu pokaonekela m’khoti kumakondweletsa mtima wa Mulungu . Kuti zimenezi zitheke , Yehova afunika kucitapo kanthu kuti acotse onse amene amakana ulamulilo wake mwadala . Baibo imayankha yokha kuti : “ Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu , ndipo ndi opindulitsa . ” — 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 . N’ciani cimene tiyenela kuganizila tikamapanga zosankha zokhudza thanzi lathu ? NYIMBO : 9 , 108 Mau a Mulungu amatitsimikizila kuti cinyengo cidzatha . 29 : 25 ) Anakhalabe wolimba mtima , cifukwa Yehova anam’thandiza monga mmene amathandizila atumiki ake onse okhulupilika . ( Ŵelengani 1 Yohane 2 : 15 , 16 . ) Kuyambila mu 2008 , takhala tikusangalala kwambili kuŵelenga Nsanja ya Mlonda yophunzila . Pambuyo pake , imbani mau a m’kaciganizoko na mphamvu ya mau imodzi - modziyo . Colinga cimeneci cinalembedwa m’malemba oyela . Magazini ino si yogulitsa . Mwina zimenezi zidzacitika mwanjila iyi : Anthu onse akuyembekeza zinthu zimene zidzawakhudza mtsogolo . 4 : 3 , 4 . 13 , 14 . ( a ) Kodi Paulo anagwilitsila nchito motani ufulu wake wokhala nzika ya Roma ? Pofika mu 2015 , ciŵelengelo ca anthu othaŵa kwawo cifukwa ca nkhondo na cizunzo cinakwela kwambili kufika pa 65 miliyoni . 121 : 1 - 3 . Kupatsa ena mlandu kumangobweletsa msokonezo na kukulitsa nkhani . “ Wopatsa Mowolowa Manja Adzadalitsidwa ” ( zopeleka ) , Nov . Potifunila zabwino , Mulungu amafuna kuti tizipindula mwa kutsatila malangizo ake . ( Mateyu 24 : 14 ; Machitidwe 1 : 8 ) Ndipo mgwilizano umene uli pakati pa atumiki a Yehova ocokela m’mitundu yonse umatheka cifukwa ca thandizo la Yehova . Kodi Yehova Mulungu na Yesu Khristu apeleka bwanji citsanzo cabwino kwambili ca kuyembekezela moleza mtima ? Aiguputo akakuona , mosakayikila anena kuti , ‘ Ameneyu ndi mkazi wake . ’ N’nayankha kuti : “ Yesu anati uthenga wabwino wa Ufumu UDZALALIKIDWA ku mitundu yonse , ndipo palibe aliyense angalepheletse zimenezi . ” Conco , tikhoza kusankha kugwilitsila nchito cinenelo potumikila ndi kutamanda Yehova . — Genesis 1 : 27 . Mulungu analenga anthu kuti azikhala padziko lapansi , osati kumwamba . Tikabatizika , timafunika kucitabe zinthu mogwilizana ndi kudzipeleka kwathu mwa kutumikila Mulungu mokhulupilika . Robert Ciranko Ena mumpingo anayambitsa magaŵano mwa kulimbikitsa anthu kutsatila Cilamulo ca Mose . “ Pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzila anga , muziwabatiza . . . , ndi kuwaphunzitsa kusunga zinthu zonse zimene ndinakulamulilani . ” — MATEYU 28 : 19 , 20 . Kodi pali phindu lanji ngati tiika patsogolo zinthu za kuuzimu ? ( Yoswa 23 : 14 ; 24 : 14 , 15 ) Ngati tikhulupilila Yehova ndi kuona mmene amatithandizila , cikhulupililo cathu cimalimba kwambili . — Salimo 34 : 8 . ( b ) a nkhosa zina ? Nanga kutsatila mfundo imeneyi kungathandize bwanji okwatilana ? 33 : 6 . ( Mlaliki 3 : 1 , 6 ) Ngati titaila nthawi yambili pa zinthu zosafunika , tingalephele kuika maganizo athu pa zinthu zofunika kwambili , zimene ndi kulambila Yehova . — Ŵelengani Aefeso 5 : 15 - 17 . Kodi Yesu anali na cidalilo cotani mwa ophunzila ake ? Ndipo anawaphunzitsa ciani ? Patapita zaka , ana ake atakula ndi kucoka panyumba , Mary anapitiliza kutumikila Yehova ngakhale kuti zinali zovuta . Kuonjezela pamenepo , tiyenela kugwilitsila nchito Baibulo pofotokoza zimene timakhulupilila , cifukwa Mau a Mulungu ali ndi mphamvu . 11 : 6 ) Koma panthawi imodzimodzi , sitiyenela kuiwala kupemphela kuti nchito yolalikila ipitebe patsogolo , makamaka m’maiko amene nchitoyo ndi yoletsedwa . — Aef . Komabe muziyesetsa kupewa maganizo otelo kuti musafooke . N’cifukwa ciani ndimakhulupilila kuti Baibulo ndi locokeladi kwa Mulungu ? Lomba nili na zaka 83 , ndipo nikali kutumikila monga mkulu . N’cifukwa ciani Yehova yekha ndiye woyenela kulamulila cilengedwe conse ? Iye anasintha dzina lake lakuti Sarai , limene liyenela kuti linali kutanthauza “ Wolongolola , ” na kum’patsa dzina lakuti Sara limene ife tonse timadziŵa . Komanso , anthu amene aloŵa kumene m’banja , nthawi zina angakangane ndi azipongozi awo , ndipo zimenezi zingakhalenso nsautso kwa iwo . 37 : 4 . Timaona uphunguwo kukhala wamtengo wapatali cifukwa umacokela kwa Yehova . Iwo akanatisiyanso , mwina sindikanakhalabe m’gulu la Yehova . ” SAMALILANI UDINDO WANU Ngakhale n’conco , wofufuza amalimbikila kukumba kuti apeze golide imeneyo . Koma bwanji ngati mumaona kuti kuŵelenga Mau a Mulungu n’kovuta ? Kodi Yakobo anakhala kholo la Mesiya cifukwa cogula udindo kwa Esau wokhala woyamba kubadwa ? Mwininyumbayo anasangalala kwambili ndipo anaganiza zopita ku Cikumbutso . Corrado ndi mkazi wake asintha zina ndi zina pa kagwilidwe ka nchito zapakhomo mogwilizana ndi kuculuka kwa nchitozo . Iwo acita zimenezi n’colinga cakuti asamakhale otopa kwambili kumapeto kwa tsiku . Pokambilana zitsanzo za m’Baibo zimenezi , tidzaona kuti kukhala odzicepetsa n’kofunika kuti ticite zinthu mogwilizana ndi cilungamo ca Yehova . Tikatelo , tidzasangalala ndi tsogolo labwino limene Yehova watikonzela . Ndinaŵelenga zonse zimene munandisiila ndipo ndinali kukuyembekezelani . ” Kodi nimaona kuti ndalama zimene nimapeza “ zonse n’zanga cabe ” ? Ndiyeno , pofuna kudziŵa ngati wopha munthu ni woyenela kum’citila cifundo kapena ayi , anafunika kupenda mosamala colinga cake , maganizo , na khalidwe lake la m’mbuyomo . Mabuku 39 oyambilila a m’Baibo analembedwa ndi Aisiraeli , kapena kuti Ayuda . Akristu odzozedwa ndi a nkhosa zina , ayenela kutsatila citsanzo cabwino ca Yesu , Mkulu wao wa Ansembe . Pofotokoza mfundo yakuti Mkhristu afunika kuganizila cikumbumtima ca ena , Paulo anati : “ Ndi bwino kusadya nyama kapena kusamwa vinyo kapena kusacita kalikonse kamene kamakhumudwitsa m’bale wako . ” Mutaphunzila mfundo zofunika za coonadi ca m’Baibulo , munalimbikitsidwa kudzipeleka ndi kubatizidwa . — Mat . Komabe , kodi tili ndi umboni woonetsa kuti Mulungu akuthandiza anthu ake masiku ano ? ( Genesis 41 : 42 - 44 ) Conco , pa tsiku limodzi cabe Yosefe anacoka m’ndende ndi kukakhala m’nyumba ya mfumu . SIKUDZAKHALANSO ZOŴAŴA , CISONI , NA IMFA Ndipo anafunikilanso kuteteza nkhosa zao ku zilombo zolusa ndi akawalala . Conco , banja lingagwilizane kuti kholo likakhale kunyumba yosungila okalamba . Komabe , cifukwa ca kuonjezeka kwa mipingo , pafunikila abale ambili kuti akalamile maudindo . Kodi cofunika n’ciani kuti dzina la Mulungu liyeletsedwe kothelatu ? Pamene ndinali wacicepele , ndinatonthozedwa kuphunzila za Atate wathu wakumwamba , amene ndi Atate wamkulu wosakhoza kufa . — Hab . Anthu ena amakhulupilila kuti . . . Iwo angafunikile kuwathandiza mwacindunji pa zinthu zina , kuwatonthoza , ndi kuwalimbikitsa ndi Malemba . Popeza kuti ndinali kudalila Yehova , ndinayamba kupemphela kwa iye mocokela pansi pa mtima . Mu 70 C.E . , asilikali aciroma motsogoleledwa ndi Kazembe Tito , anabwelela ndi kuononga Yerusalemu . ( Yobu 31 : 1 , 7 , 9 ) Tifunika kuyesetsa kulamulila maso athu kuti tisayang’anitsitse munthu wina mosayenela . Koma dipo la Khiristu sikuti idzangobweletsa cabe madalitso amtsogolo ku mtundu wa anthu ayi . Ndipo Yesu nayenso ndi wofunitsitsa kuthandiza . Nditayamba kuphunzila Baibulo , ndinazindikila kuti ndifunika kusintha umoyo wanga . Potsiliza anakamba kuti : “ N’nazindikila kuti niyenela kukhala pa ubwenzi wolimba na Yehova . Mwa kumvela malangizo a m’Baibo , timalimbikitsa ciyelo , mtendele , na mgwilizano mumpingo . Conco pamene anali acinyamata , io sanaphunzitsidwe kuika coonadi patsogolo m’moyo wao . — Mat . Kwa zaka zoposa 200 , Aisiraeli anali akapolo ku Iguputo . Posacedwapa , angelo adzasiya kugwila mphepo zoononga za cisautso cacikulu . Komanso , kuyamikilidwa kapena kutamandidwa mopambanitsa kungabweletsenso ciyeso pa kudzicepetsa kwathu . Conco , tingathe kuona kuti Isaki anali munthu wokoma mtima ndi wacifundo . Ndipo mamvekedwe ena anali kusonyeza kuti asilikali afunika kumenya nkhondo . Kwa masiku 40 , Yesu woukitsidwayo anaonekela kwa ophunzila ake m’munda umene unali pafupi ndi manda ake . Anaonekelanso kwa ophunzila ena panjila ya ku Emau ndi kumalo ena . Kucita izi kumaonetsa kuti afuna kutsogoleledwa na Mulungu komanso na Mwana wake . Pa 1 Yohane 3 : 1 timaŵelenga kuti : “ Taganizilani za cikondi cacikulu cimene Atate watisonyeza . ” [ Mau apansi ] Zimenezi zinaphatikizapo kuphunzitsa anthu kuopsa kokoka fodya , kuletsa makampani kupanga fodya wambili , kuonjezela msonkho wake , ndi kukhazikitsa mapulogalamu othandiza anthu kuti aleke kukoka . Yehova amayankha mapemphelo na mapembedzelo athu ocokela pansi pamtima . Kodi pali kusiyana kotani pakati pa cidziŵitso , kumvetsa zinthu , ndi nzelu ? Sara anali kum’konda ngako mwamuna wake . N’cifukwa ciani tingati Aroma caputa 8 ni yofunikanso kwa aja odzakhala padziko lapansi ? Mariya sanakhalebe wodabwa , ndipo mwaulemu anayankha kuti : “ Ndinetu kapolo wa Yehova ! Ndiponso sitiyenela kupeputsa nchito yathu ‘ cifukwa cakuti tinayamba kumanga ndi zinthu zocepa . ’ ( Genesis 5 : 21 - 23 , 25 ) Kodi awa ndiwo anali mapeto a moyo wake ? Nyimbo ya Solomo imafotokoza bwino kwambili za cikondi cimene cingakhale pakati pa mwamuna ndi mkazi . Monga mmene citsanzo ca Julien cionetsela , tiyenela kunyalanyaza zofooka za ena . Tiyenela kuona zabwino mwa io ndi kuyamikila maluso ao . Umu ndi mmene Yesu anacitila ndi mtumwi Petulo . ( Onani pikica namba 3 kuciyambi . ) ( b ) Kodi akazi okhala na mapiko anapita naco kuti ciwiya copimila ? 20 : 29 , 30 ; 2 Pet . 2 : 2 , 3 ; Yuda 3 , 4 ) Malinga n’zimene Yesu anakamba , mpatuko umenewu wocititsidwa ndi “ woipayo , ” Satana , unali kudzakula ndi kudzalepheletsa anthu kudziŵa cipembedzo coona kufikila “ mapeto a nthawi ino . ” ( Mat . M’dzikoli , anthu ambili amalephela kudziletsa ndipo amasangalala ndi ciwelewele . Popeza kuti Mulungu ndi Yesu ndi okonzeka kusintha maganizo ao , ifenso tiyenela kuganizila zifukwa zimene zapangitsa munthu kucita zinthu mwa njila ina yake ndi kusintha maganizo athu . CAKA COBADWA : 1952 12 : 25 ) Maliko anafunikila kusamalila Paulo ndi Baranaba paulendo wao woyamba waumishonale . Mtumwi Paulo anapeleka cenjezo lofanana ndi limeneli kwa abale ndi alongo ake odzozedwa . ( Ŵelengani Afilipi 3 : 7 , 8 . ) Komanso , tonsefe timamvela malangizo a m’Baibulo amene amatithandiza kutamanda Yehova mogwilizana Komabe , nthawi zina Yehova amatidalitsa m’njila imene sitinali kuyembekezela . Mulungu ali ndi dzina limene amadziwika nalo . Mofanana ndi Paulo , aliyense ayenela kusinkhasinkha pa zinthu zimene Yehova wam’citila . Njila yabwino koposa ndiyo kukambilana kaŵilikaŵili ndi ana anu . Mwacitsanzo , timafunikila cakudya , zovala , na malo okhala . N’zosadabwitsa kuti msonkhano wacigawo umenewu , umene unacitika mu 1922 ku Cedar Point , Ohio , wakhala wosaiŵalika m’mbili ya atumiki a Mulungu . * Kofikila sitima zapamadzi kunali kutaimilila Ophunzila Baibo 12 , amene anabwela kudzalandila M’bale Russell . ( b ) Kodi kulefuka kunam’khudza bwanji Paulo ? Mkazi wanga anali atagona pampando kuti apumuleko uku tikukambilana mmene tsiku layendela . Cifukwa cakuti anafuna kupatsa anthu ufulu wakuti azidya nyama . Kapena kodi mtundu umabadwa nthawi imodzi ? Conco , m’maŵa ndisanapite m’kalasi ndinali kucita mapemphelo ochedwa namazi . Amalalikila pa mpata uliwonse umene apeza . Pofotokoza mfundoyi Paulo anati : “ Cikondi cimene Kristu ali naco cimatikakamiza , cifukwa tatsimikiza kuti munthu mmodzi [ Yesu ] anafela anthu onse , . . . Kodi ndinu wofunitsitsa kukapezekapo pa Cikumbutso ca caka cino ? Amakhala na mtendele wa m’maganizo , amatha kukhala na mabwenzi abwino , ndipo sakhala aukali , ankhawa kwambili , kapena ovutika maganizo ngati mmene amakhalila anthu osadziletsa . Mpaka lelo , anthu mamiliyoni ambili amafa ndi matenda a AIDS , TB , na maleliya , ngakhale kuti a zacipatala ayesa - yesa kufufuza mankhwala . ( Mlaliki 3 : 11 ) Popeza kuti zili conco , kodi zingakhale zomveka kuti Mulungu wacikondi atipatse cinthu cimene sangathe kucikwanilitsa ? 10 : 3 - 6 ; Akol . Ngakhale pamene anali kumanga cingalawa , cimene mwina cinatenga zaka 40 kapena 50 kuti cithe , Nowa anapitiliza kuika zinthu zauzimu patsogolo . 4 : 4 - 9 , 17 - 22 . 2 : 1 - 5 . PA MATEYU 13 : 24 - 26 , Yesu anati : “ Ufumu wakumwamba uli ngati munthu amene anafesa mbeu zabwino m’munda wake . Koma anthu ali m’tulo , kunabwela mdani wake . Tikamagwila mwacangu nchito imene Mulungu anatipatsa , sicidzakhala covuta kuyembekezela thandizo lake . Tiyeni tikambilanenso njila ina imene tingakonzekelele kudzakhala ndi moyo weniweni umene ukubwela . M’baleyu anali kuyenda m’maiko osiyanasiyana padziko lonse lapansi n’colinga cokalimbikitsa abale ndi alongo ake akuuzimu . Iye anali kumasuka kuceza ndi aliyense pa Beteli ndiponso anthu ena amene anali kufuna kuceza naye , kupempha uphungu kapena thandizo lina lililonse . ( b ) Tingawaphunzitse bwanji ana athu ndi acatsopano kucita zopeleka kuti nawonso alandile madalitso ? Komiti Yoona za Nchito Yolemba Mabuku Ana amenewa ndi akazi ao anapita kukaona makolo ao ku Japan , kuti akaone mmene angathandizile . Conco , tinayamba kuonetsa cikhulupililo mwa Yesu . Kuika patsogolo zinthu zauzimu kudzawonjezela cimwemwe m’banja mwanu ( Onani ndime 17 ) Kodi abale a ku Japan analandila mphatso yosangalatsa yotani ? ( Vesi 6 - 26 ) N’zoona kuti zinthu zimenezi zakhala zikucitika kwa zaka zambili . Pamene M’bale Russell na anzake anali kudutsa cakufupi ndi matauni na midzi yokongola , anazindikila kuti mbeu za m’munda wauzimu kumeneko zinali “ zitaca kale ndipo zinali kuyembekezela okolola . ” Ganizilani izi : Pambuyo pa imfa ya Yesu , Akristu ambili amene anali Ayuda anali kutsatila Cilamulo kwambili ndipo anavutika kuti aleke kucitsatila . 4 Zoona Zake Ponena za Angelo Ndi zinthu zina ziti zimene zingatithandize kusankha mau abwino ? Ngati tifuna kuthandiza ena kupita patsogolo , tifunika kukhala maso . ( Luka 18 : 1 - 7 ) Amamvetsela mapemphelo athu cifukwa amatikonda . Abale ake anali kumuda kwambili cifukwa ca nsanje cakuti anamugulitsa monga kapolo . Baibulo limanena mosapita m’mbali kuti Satana adzatsekeledwa kuphompho kwa zaka 1,000 , osati kudyedwa kapena kuikidwa m’manda . — Chiv . 30 : 7 , 8 ) Yehova anayankha mapemphelo a Davide . Ngati timapemphela modzicepetsa , moona mtima , ndi moyamikila , mapemphelo athu nafenso adzakhala ngati zofukiza , ndipo Yehova adzakondwela nao . — Chiv . ( 1 Akorinto 15 : 3 , 4 ) Patapita nthawi anakhala Mfumu ya Ufumu wa Mulungu . “ Ndidziŵa Kuti Adzauka , ” Dec . Cotelo ngati inuyo , . . . mumadziŵa kupeleka mphatso zabwino kwa ana anu , kuli bwanji Atate wanu wakumwamba ? Ndithudi , iye adzapeleka zinthu zabwino kwa onse om’pempha ! ” Timasangalala ngati ena atikhululukila . Masiku ano , a “ kagulu ka nkhosa ” amene ali na ciyembekezo copita kumwamba , ndi a “ nkhosa zina ” amene ali na ciyembekezo codzakhala pa dziko lapansi , ni “ gulu limodzi ” la anthu a Yehova amene iye amawakonda . ( Luka 12 : 32 ; Yoh . 4 : 7 ) Tatsala pang’ono kukumana na cisautso cacikulu cimene sicinacitikepo pa dzikoli . Yesu ananena kuti : “ Idzafika nthawi pamene onse ali m’manda acikumbutso . . . adzatuluka . ” — Yoh . 5 : 28 , 29 . Komabe , mwamuna wina dzina lake Edwin amayetsetsa kutengela citsanzo ca Yesu . ( a ) Pangano la Cilamulo linapeleka mwai wotani kwa Aisiraeli ? Mtumwi Petulo analangiza Akristu kuti : “ Monga ana omvela , lekani kukhala motsatila zilakolako zimene munali nazo kale pamene munali osadziŵa . Koma khalani motsanzila Woyela amene anakuitanani . Inunso khalani oyela m’makhalidwe anu onse , cifukwa Malemba amati : ‘ Mukhale oyela , cifukwa ine ndine woyela . ’ ” ( 1 Pet . Koma kodi mumadziŵa kuti tilinso ndi pulogalamu yophunzitsa Baibulo padziko lonse ? Pambuyo pa zaka zambili , anthu ena anasankha kukhala okhulupilika kwa Yehova . Ndiponso , Ophunzila Baibulo ndi mabanja ao anatukonda kwambili tumabuku twa zithunzithunzi tumenetu . Ngakhale n’telo , Yesu anali kudziŵa kuti moyo ndiye wofunika kwambili kuposa cakudya , ndipo thupi n’lofunika kwambili kuposa covala . 36 : 7 ) Apa n’zoonekelatu kuti Naboti anali kulemekeza malamulo a Yehova . ( Salimo 78 : 69 ) Conco , mfundo yocititsa cidwi imeneyi ionetsa kuti ngakhale mbali yocepa kwambili ya m’Cilamulo singapite pacabe osakwanilitsika . Laciŵili ndi Agalatiya 2 : 20 . ( Levitiko 19 : 18 ) Ndiyeno , kodi mau a m’lemba la Ekisodo amatanthauza ciani ? Kodi Yehova ndi Yesu ali ndi mphamvu yocita ciani ? Nanga tikambilana mafunso ati ? Mosiyana ndi maganizo amenewo , Yehova amanenedwa kuti ndi “ Mulungu wacoonadi , ” ndipo anakamba kuti “ sindinasinthe . ” Kodi zotsatilapo zake zinali zotani ? Mu ulaliki . Ngakhale zinali conco , usakhale mlandu kwa io . ” Komabe , Paulo anadziŵa kuti sanali yekha . Munthu amapanga mapulani kapena zolinga mogwilizana ndi zimene zili mumtima mwake . Conco , Mkhristu aliyense afunika kudzifufuza nthawi na nthawi kuti adziŵe ngati amaona zinthu zimenezi moyenela . Angacite zimenezi mwa kudzifunsa kuti : ‘ Kodi nimaona zinthu zakuthupi kukhala zofunika kwambili , cakuti nimathela nthawi yaitali kufufuza na kuganizila za mamotoka amakono , kuposa nthawi imene nimathela pokonzekela misonkhano yampingo ? Mwacitsanzo , wina angatiuze kuti zinthu zacisoni zimene zinam’citikila zinacititsa kuti azikaikila ngati Mlengi wacikondi aliko . Koma timadwalabe ndi kukalamba . Kodi mabwenzi anu amakhudza bwanji unansi wanu na Yehova ? Panthawiyo , “ Petulo anaimilila pamodzi ndi atumwi 11 ” ndi kuyamba kuphunzitsa coonadi copulumutsa moyo kwa khamu la Ayuda ndi anthu otembenukila ku Ciyuda . ( Mac . Mofanana ndi anthu ambili amene amafuna thandizo la Mulungu , Mfumu Davide anali kukumana ndi mavuto kaŵili - kaŵili . 4 : 10 ) M’pemphelo lake locokela pansi pa mtima , usiku wakuti maŵa lake aphedwa , Yesu anatsimikiza kuti sadzasunthika pa cifunilo ca Mulungu . Popeza ndife ophunzila Baibulo , kodi tingaphunzile ciani tikaona mmene anthu amepezela golide ? Nthawi zina , tingaone ngati zopeleka zathu zocepa sizingathandize kweni - kweni . Akalephela kukwanilitsa zolinga zawo , amaleka zimene anali kucita pofuna kuzikwanilitsa . Popeza ndife opanda ungwilo , nthawi zina timasemphana maganizo ndi abale ndi alongo athu . Nthawi zonse muzikumbukila lonjezo lolimbikitsa ili la Mulungu : “ Ndikulenga kumwamba kwatsopano ndi dziko lapansi latsopano . Linki ya peji imene pali malamulo a Kaseŵenzetsedwe ka mawebusaiti athu ili pansi pa peji yoyamba ya jw.org . Malamulo amphamvu amene ali pamenepo akhudza ciliconse cimene cili pa mawebusaiti athu . Tsiku na tsiku pali zinthu zambili zimene timafunika kucita komanso zina zambili zimene ise tingakonde kucita . Ganizilani za Mwiitiyopiya wotembenukila ku Ciyuda amene anali pa ulendo wobwelela kwawo kucokela ku Yerusalemu , kumene anapita kukalambila . Ngakhale kuti anagonjetsa aneneli a Baala okwanila 450 , Eliya anathaŵa pamene anamva kuti Mfumukazi Yezebeli anali kufuna kumupha . ( Aroma 8 : 15 - 17 ) Kwa ife a “ nkhosa zina , ” zili monga kuti Yehova walemba dzina lathu pa satifiketi yotivomeleza kukhala ana ake . Hopkinson ) , Dec . Pambuyo pakuti Ufumu wa Mulungu walamulila zaka 1,000 padziko lapansi la paradaiso , angelo oipa amenewo adzapatsidwa kanthawi kocepa kuti ayese anthu komaliza . Wina anali kukonda kukalipila mnzake . M’kupita kwa nthawi , iye anayenelela kutumikila monga mtumiki wothandiza , ndipo tsopano ndi mpainiya . Ine na mlongosi wanga wamkulu , Dorothy , tinali kucotsedwa m’kilasi panthawi ya miyambo imeneyi . Abulahamu anauza Sara kuti : “ Fulumila ! Nthawi ina Yesu anapemphela usiku wonse . Kodi iye akanacita zimenezo akanadziŵa kuti Yehova samvela mapemphelo ? Patangopita nthawi yocepa kucokela pamene anacita msonkhano mu 49 C.E . , Petulo anapita ku Antiokeya wa ku Siriya . N’cifukwa cake ndakumbukila inu . ” “ Iye Amacititsa Kuti Kukhale ” Baibulo limati : “ Pitilizani kukonda akazi anu monga mmene Kristu anakondela mpingo . ” Atate ataimilila pa kona m’mbali mwa mumseu , akugaŵila magazini kwa anthu opita Davide 19 - 21 . ( a ) N’ciani cofunika cimene timacita poonetsa kuti “ ndife ziwalo za thupi limodzi ” ? Conco , tinayamba kukhala ndi banja lina la Mboni pamudzi wina waukulu . YEHOVA MULUNGU anati : “ Kumwamba ndiko mpando wanga wacifumu , ndipo dziko lapansi ndilo copondapo mapazi anga . ” ( Yes . Mofanana ndi asilikali ena atsopano , ndinapatsidwa mlungu umodzi wakuti ndiphunzitsidwe ndi kuzolowela nyengo ya kumeneko . 6 : 4 ) Kodi udindo umenewu ndi wopepuka ? Ndipo zimenezi n’zofunika kwambili m’cikwati . Abweletse mboni zao kuti akhale olungama ndipo mbonizo zimve ndi kunena kuti , ‘ Zimenezo ndi zoona ! ’ ” — Yes . Ngati wina wakucitilani nkhanza kapena zinthu zina mopanda cilungamo , n’ciani cingakuthandizeni kulamulila mkwiyo wanu ndi kucita zinthu m’njila yokondweletsa Yehova ? Ine ndi akaidi ena mahandiledi ambili , tinaikidwa m’kampu imene munali citetezo cocepa . * Liu lake lenileni lili m’zilembo zakuda , ndipo mphatikila zake zinalembewa m’zilembo zanthawi zonse . Cisudzulo cinali kuloledwa , koma panali malamulo ake . Iye anati : “ Khalidwe limeneli n’loipa cifukwa umakhala na mzimu wadyela kwambili . ” Ndipo Baibulo silikambapo ciliconse pa sitaelo ya zovalazo . 8 : 23 ) Koma kusiyana kwa zitundu kungapangitse kuti cikhale covuta kwa makolo kuphunzitsa ana awo coonadi . Pambuyo pake , Corinna nayenso anam’tenga ndi kupita naye ku Siberia , kutali kwambili ndi kwao . Ngati tikhutilitsa zosoŵa zathu zakuuzimu , cikondi cathu pa Yehova cimakula ndipo timakhala ndi cimwemwe . Njila ya Kumoyo Wamuyaya — Kodi Mwaipeza ? Mogwilizana ndi ulosi umenewu , kuciyambi kwa October , 539 B.C.E . usiku , kunacitika cinthu cimene cinagwedeza dziko lonse . Okwatilana amene amatumikila Yehova , samaona cikwati kukhala mgwilizano wamba . Ndipo ngati napita kusukulu , n’nali kumwa mowa atica akatuluka m’kalasi . Conco kuyamikila zimene Mulungu waticitila ndi kukhulupilila kwambili malonjezo ake kuyenela kutilimbikitsa kucita zimene tingathe kuti tiyenelele kudzaloŵa m’dziko latsopano . 3 : 28 . Yehova amadziŵa zimenezi , ndipo amafuna kutithandiza kugonjetsa zizoloŵezi zoipa zimene tingakhale nazo . ( 1 Maf . N’nawayankha kuti : “ A dokota , ndine wodwala mwauzimu osati mwakuthupi . Koma sindikuonabe kugwilizana ndi caka ca 1914 . Kumathandiza mipingo kukhala yogwilizana , ndipo zimenezi zimapangitsa kuti Yehova alemekezeke . Anthu amakonda kucita zaciweleŵele , zacinyengo , ndi zankhanza . 9 - 11 . ( a ) Kodi ena amakumana ndi mavuto otani ? Malamulo ake amatipindulitsa . Fotokozani cifukwa cake wothaŵa anali kukhala wotetezeka ndi wacimwemwe mumzinda wothaŵilako . Kodi iwo anacitanji ? Komabe , kodi munaganizilapo ngati Akhristu a m’nthawi ya atumwi , amene anali anzake a Yesu anali kukondwelela Khrisimasi ? Tikakumana ndi vuto linalake , tifunika kuganizila mfundo za m’Baibo zokhudzana ndi nkhaniyo ndi kuziseŵenzetsa m’njila yoyenela . Koma mu 66 C.E , pamene bwanamkubwa waciroma ku Yudeya , dzina lake Gessius Florus analanda ndalama zocokela m’thumba la kacisi wopatulika , Ayuda okwiya anafika polema nazo . Fotokozani cifukwa cake cikhulupililo si maganizo cabe . Federico atakumana ndi vuto , mnzake Antonio anamumvetsela ndi kumulimbikitsa Komabe , cikhulupililo ceni - ceni ni “ ciyembekezo cotsimikizika ” cimene Akhiristu ali naco . ( Aheb . 15 : 21 ) Komanso Akristu oyambilila anali kusonkhana m’nyumba za abale ndi alongo . ( Mac . Komabe , mu 1915 pa magulu 86 amene anakhazikitsidwa , magulu 14 ndi amene anali kuonetsa seŵelo limeneli nthawi zonse . Cakudya cimene anali kutipatsa cinali cabwino . 6 : 4 ) Ifenso tifunika kudziŵa zimenezi , cifukwa masomphenyawa amatikhudza . 1 PEWANI “ MZIMU WA DZIKO . ” — 1 Akor . Kenako asilikali a Aroma akuyamba kugwetsa linga la kacisiyo . Baibo imatilimbikitsa ‘ kukhala ofulumila kumva , odekha polankhula . ’ Masiku ano , amuna 6 onyamula zida zophwanyila aimila gulu la angelo lotsogoleledwa ndi Yesu . Nkhani ya ubatizo , imene imakonzedwela maka - maka opita ku ubatizo , ni mbali yofunika kwambili pa msonkhano uliwonse wadela ndi wacigawo . Pambuyo pake , n’napita ku sukulu ya boding’i . Pokamba za Yehova , wamasalimo anati : “ Iye amateteza moyo wa anthu ake okhulupilika . Amawalanditsa m’manja mwa anthu oipa . ” Nkhani ina ingafalitsidwenso ngakhale kuti poyamba inadziŵika kuti ndi yabodza . Ndipo tonse tinaweluzidwa kuti tikhale m’ndende zaka ziŵili . Ulosi umenewo unaonetsanso kuti anthu a m’nthawi imeneyo adzawonongedwa pamene Yehova adzabwela ndi “ miyandamiyanda ya oyela ake . ” Oyela amenewa ndi magulu a angelo okonzeka kumenya nkhondo kuti awononge anthu oipa . Kodi tifunika kucita ciani “ tsiku ndi tsiku ” ? Nanga n’cifukwa ciani ? Anthu amene adzapezekamo adzasangalala ndi paradaiso komanso ubwenzi na Mulungu , zimene Adamu anataya . — Chivumbulutso 21 : 3 . Mwa cisomo ca Mulungu , macimo athu anakhululukidwa , ndipo angapitilizebe kukhululukidwa . ( 1 Mafumu 18 : 41 ) Pambuyo pophunzila zitsanzo zimenezi , dzifunseni kuti : ‘ Kodi cikhulupililo canga n’colimba monga ca Eliya ? ’ M’bale wina dzina lake Juan , amene anapita kukatumikila ku Mexico , anati : “ Zimakhala monga kuti wabadwanso , ndipo umafunikila kupanga mabwenzi atsopano . Colinga ca Mulungu cimeneci cidzakwanilitsidwa . Iye amakhala wotsimikiza ndi mtima wonse kuti wasankhidwa kuti adzapite kumwamba . Koma patapita milungu iŵili pambuyo pokwatilana , mwamuna wake anamuletsa kupita ku misonkhano yacikristu . Popeza mumaphunzila Baibulo , mayankho ena a mafunso amene ali m’nkhani zimenezi mukuwadziŵa . Gulu la nkhondo la Sisera linali la mphamvu , ndipo linali ndi magaleta 900 amene anali ndi zitsulo zazitali zakuthwa m’mawilo ake . Koma nthawi zina , anali kumvetsela ndipo anali kufuna kuphunzila zoonjezeleka . Ndiponso acinyamata ena anali kufuna kukhala ndi zolinga za kuuzimu , koma makolo ao anawalimbikitsa kucita maphunzilo apamwamba . Kaya amene si Mboniyo adziŵe kapena asadziŵe , iye “ amayeletsedwa ” cifukwa cokwatilana ndi wokhulupilila . Mfundo yaciŵili ndi yakuti , Yesu amafuna kuti tonse tizicita khama pogwila nchito yolalikila . Cenjezo limene lili m’fanizo la anamwali 10 limaonetsa kuti Yesu nayenso anali ndi cidalilo cakuti odzozedwa adzalandila mphoto yao . Anthu ambili zawacitikilapo . ( a ) M’fanizo la Yesu , n’cifukwa ciani zipatso sizitanthauza ophunzila atsopano ? ( Ŵelengani Yakobo 1 : 22 - 25 . ) Amapezanso njila zowathandiza kupilila . Ahabu anafa pankhondoyo , koma Yehosafati anapulumuka ngakhale kuti anatsala pang’ono kuphedwa . Iwo anabatizika mu 1914 , apo n’kuti ali ndi zaka 17 . Kodi dokota angatithandize bwanji ngati sitinapite kukamuuza vuto lathu ? Ndipo amadziona kuti ni a Mboni za Yehova . Iwo anali atagwila mwamphamvu mphepo zinai za dziko lapansi . ” ( Chiv . Baibulo limati pamene Danieli anali ku Babulo , “ anatsimikiza mumtima mwake kuti sadzidetsa ” mwa kupewa cinthu ciliconse cogwilizana ndi kulambila konama . Kodi iye afunika kucita ciani ? N’ciani cinapangitsa ofalitsawo kukhala na colinga cokukila ku dzikolo ? Kodi muganiza kuti mayiyu anaona kuti Yehova anayankha pemphelo lake ? Ine ndine Yehova . ” 13 : 3 , 7 . Anthu ambili m’dziko la Satanali amakamba “ mau owawa ” amene ali ngati “ mivi ” kapena “ lupanga ” pofuna kukhaulitsa anzao kapena kuwakhumudwitsa . ▪ “ Cipulumutso Canu Cikuyandikila ” 71 : 9 ) Posacedwapa , tonse tidzayamba kukula koma osakumana ndi mavuto alionse a ukalamba kapena kuti masiku oipa . Conco , Paulo anapelekedwa ku Kaisareya . Yehova amatiumba mwa kuseŵenzetsa Baibulo , mzimu wake woyela , ndi mpingo . Iye adzaonetsetsa kuti zathetsedwa mwamsanga . ( 1 Akor . ( Maliko 9 : 33 - 37 ) Akulu angatengele citsanzo ca Yesu mwa kulangiza ena mokoma mtima . — Agalatiya 6 : 1 . Musalole mkwiyo kukulamulilani . Anthu ambili amatsutsa mfundo yakuti Satana aliko . ( Hos . 14 : 2 ) Inde , nthawi ya kulambila kwa pabanja iyenela kukhala yosangalatsa kwa onse m’banja , “ pakuti cimwemwe cimene Yehova amapeleka ndico malo anu acitetezo . ” — Neh . Yehova anaika Mwana wake “ pamwamba - mwamba kuposa boma lililonse , ulamulilo uliwonse , amphamvu onse , ambuye onse . ” Yehova ndi amene amamvetsa nkhawa zathu kuposa wina aliyense . Ungam’pemphe kuti afotokoze mmene moyo unayambila popanda Mlengi . Mmodzi wa anthuwa anali Abulahamu . Cifukwa cokana kunyamula zida za nkhondo , analamulidwa kukapika jele kwa miyezi 10 m’ndende yochedwa Kingston Penitentiary ku Ontario , ku Canada . ( Gen . 15 : 13 ) Esau anaonetsanso kuti anali kukonda zinthu zakuthupi ndi kusayamikila zinthu zopatulika , mwa kukwatila akazi aŵili a mitundu ina . Ganizilani citsanzo ca Baranaba ndi Maliko . ( Mac . Kwa zaka zambili , iye wakhala wotamandika kwambili . Iye anakhalako Yehova akalibe kupatsa Aisiraeli Cilamulo , ndipo kukali zaka zambili Yesu akalibe kutifela . Zinthu zikafika apa umasoŵa cocita . Sitikudziwa kuti mfumu idzagwilitsila nchito ciani kuti iononge dziko loipali . Gary , wa ku North Carolina , anali kugwila nchito yoyang’anila zomangamanga kwa zaka 30 asanapite ku Warwick . Si kuti Mulungu adzakondwela nanu kapena kukudalitsani mwapadela cifukwa cakuti mwapanga ulendo wautali wopita ku tuakacisi . Nthawi zambili , zimene timakonda zimaonetsa zimene zili mumtima ndi m’maganizo mwathu . Conco , kuti tilimbitse cikhulupililo cathu , tinali kuyesetsa kupeza mpata wokumana pamodzi kuti tiphunzile Baibo , kuimba nyimbo zauzimu , ndi kupemphela . Mulungu wanga adzandimvela . ” “ Ngakhale kuti mwana wathu anafa pa ngozi ya ndeke , tikali kukumbukila nthawi imene tinali kusangalalila pamodzi . ” — Robert ( Sal . 144 : 15 ; Yoh . Umu ndi mmene mtumikiyu akufotokozedwela m’nkhani ino . — Genesis 15 : 2 ; 24 : 2 - 4 . Izi n’zimene Ricardo anacita . Iye anati ; “ Ndikadziŵa kuti mkazi wanga angakhumudwe , ndimasamala kakambidwe kanga kuti ndisamukhumudwitse . ” Masiku ano , atumiki ena a Yehova ali ndi cakudya ca kuuzimu coculuka kuposa ena . Amenewo anacoka pakati pathu , koma sanali m’gulu lathu . . . Lomba ganizilani citsanzo ca Mariya . Koma anthu ambili sadziŵa colinga ca moyo . 21 : 11 - 13 ; 2 Maf . Kuti tipeze yankho , tiyenela kudziŵa kuti fanizoli likunena za nthawi iti . Mu January 1949 , tinakwatilana . 15 : 28 ) Colinga ca ulamulilo wa Mwana cidzakwanilitsidwa . Zioneka kuti pakati pa otsatila a Yesu panalinso akazi olemela . Nkhani yotsatila m’nkhani zimenezi idzafotokoza mavesi a m’Baibulo amene amatiunikila kuti tidziŵe utali wa nthawi zokwanila 7 . Tingaonetse bwanji kuti timalemekeza makonzedwe a Yehova opelekela cilango kwa anthu osalapa ? Kulumbila m’dzina la Yehova ni nkhani yaikulu ngako . Pa mbali imeneyinso , akulu ayenela kutengela citsanzo ca m’Baibo ca mmene tingapelekele uphungu m’njila yolimbikitsa . 8 , 9 . ( a ) Magazi okhetsedwa a Yesu anakwanilitsa ciani ? Adamu anafa pamene Inoki anali na zaka 308 . Anandiitanila ku msonkhano wa Mboni . Conco , kunali koyenela kuti Akhiristu a ku Roma adzifufuze kuti aone zinthu zimene anali kuika patsogolo . Kenako Yehova analanga Eli ndi ana ake aŵiliwo . Koma mwina mungafunse kuti , ‘ N’cifukwa ciani sanali kuyang’ana pa Baibulo lake poŵelenga ? ’ Kalatayo ndi imene tsopano imachedwa buku la Aheberi m’Baibulo , ndipo inalembedwa n’colinga colimbikitsa Akristuwo kuti adzathe kupilila mavuto amtsogolo . Mpake kuti Yehova anamucha “ mtumiki ” wake . Kuwonjezela apo anakamba kuti : “ Iyetu ndi munthu wopanda colakwa ndi wowongoka mtima , woopa Mulungu ndi wopewa zoipa . ” — Yobu 1 : 8 . Ndiponso , Aisiraeli anakhala mboni zakuti Yehova ndiye Mulungu woona ndi kuti amakwanilitsa malonjezo ake . Anaonjezelanso kuti : “ Ndikuyamikila kwambili kuti Yehova ndi Mulungu wanga . ( Mateyu 6 : 24 ) Ndithudi , n’zosatheka kutumikila Yehova mwacimwemwe kwinaku tikufunafuna zinthu za m’dzikoli . Adzadabwa kwambili kuona kuculuka kwa Malemba amene amakamba za iye na mbadwa zake . Alondawo anali kukamba zimenezo ngakhale kuti munthuyo anali kuoneka wathanzi ndithu , wosadwala . Ndipo malinga n’zimene taphunzila pa nkhani ya Yosefe , tifunika kupewa kukamba zoipa za ena cifukwa kucita zimenezi sikungathetse vuto . Iwo amaganiza kuti adzaleka kugwila nchito yamanja akadzapeza nchito ina yabwino . ” Zimene zinamuthandiza kupilila ni zimene n’namuuza zokhudza zomwe n’nakumana nazo m’ndende . Ndipo cakumapeto kwa utumiki wake , iye analembela kalata Akhristu anzake . Posacedwapa , Kristu adzapambana nkhondo yolimbana ndi dziko loipali pa Aramagedo . 3 : 16 ) Nsembe ya Yesu ndi umboni wakuti iyenso amatikonda . Akuluakulu a asilikali ndi a boma anadabwa ndi mgwilizano umene anaona pamsonkhano . Conco , ngati omasulila acotsa dzina la Mulungu m’Mabaibulo ao , ndiye kuti salemekeza Yehova . Iye anati : “ Inu nthawi zonse mumasunga mapangano . ” ( Sal . Mwacitsanzo , mungayese kudziŵa mmene ana anu amaonela utumiki . Panthawi ina izi zitacitika kale , mwacimwemwe M’bale Rutherford anapatsa moni M’bale Klein kuti , “ Bwanji M’bale Karl ! ” Conco , kuyambila nili wamng’ono , n’nayamba kulakalaka kuphunzila mfundo zambili za m’Baibo , monga zimene n’naŵelenga m’mabuku ocititsa cidwi amenewo . Ndinadziŵa kuti imfa ndi cisoni zidzatha cifukwa Yehova adzaukitsa akufa . Pomvela mau a Yesu , munthuyo ananyamuladi macila ake ndi kuyamba kuyenda . Ampatuko na otsutsa ena amafuna kuseŵenzetsa zofalitsa zathu pa ma webusaiti awo kuti asoceletse Mboni za Yehova ndi anthu ena . Nanga bwanji za nkhani yosunga ndevu kwa abale ? ( 1 Petulo 2 : 23 ) Ndiye cifukwa cake , nthawi zonse timadzicepetsa ndi kumvela malangizo akuti : “ Osabwezela coipa pa coipa kapena cipongwe pa cipongwe , koma m’malomwake muzidalitsa . ” — 1 Petulo 3 : 8 , 9 . Komiti Yoona za Nchito Yophunzitsa M’bale C . Koma Yehova sanasinthe ciweluzo cake pa Ahabu . ( Aheb . 11 : 7 ) Conco , n’zosadabwitsa kuti iye anali kunyozedwa , kutsutsidwa , ngakhale kuwopsezedwa . Baibo imafotokoza cikondi momveka bwino kuti : “ Cikondi n’coleza mtima ndiponso n’cokoma mtima . Mwacitsanzo , Paulo anakamba kuti Melekizedeki anali kuimila Yesu , koma sanakambe ciliconse pankhani yakuti panthawi ina Melekizedeki anapatsa Abulahamu mkate ndi vinyo kuti asangalale pambuyo pogonjetsa mafumu anai . Hutter anafuna kuwonjezelapo Malemba Acigiriki Acikhristu omasulidwa m’Ciheberi . Kukhala acikondi na okoma mtima kudzatithandiza kupewa kucitila nsanje anthu ena . Kodi iwo anali na cikhulupililo monga ca Marita , amene anakamba kuti : “ Ndikudziŵa kuti [ mlongosi wanga ] adzauka pa kuuka kwa akufa m’tsiku lomaliza ” ? Nyengo ya Cikumbutso ndi nthawi yabwino yoganizila mmene tingathandizile abale ndi alongo mumpingo wathu , makamaka okalamba . 20 : 7 , 8 ) N’ciani cidzawasonkhezela kucita zimenezi ? Kuyamikila munthu n’kothandiza . Kodi mungafunike kucepetsa nthawi imene mumathela pocita zosangulutsa ? — Ŵelengani Aefeso 5 : 15 , 16 . Kodi cikumbumtima cathu cimatilimbikitsa bwanji kulalikila ? 8 : 28 ) Iye anali kufuna kuti anthu ena adzipindulanso ndi zimene anaphunzila . Cifukwa ca zimenezi , m’maiko ena lemba la “ Yohane 3 : 16 ” kapena mau ake , nthawi zambili amalembedwa pa zocitika zosiyana - siyana , pa zomata pa magalimoto , ndi pa zinthu zosiyana - siyana . N’cifukwa ciani kulemekeza Yehova na Khristu n’kofunika kwambili ? ( Aroma 3 : 23 ) Koma mwa kupitiliza “ kumenya nkhondo yabwino yosunga cikhulupililo , ” tingapambane pankhondo yolimbana ndi matupi athu opanda ungwilo . — 1 Tim . Ndipo kuzengeleza kubatizika kungaononge ubwenzi wa munthu na Yehova . ( Yak . Onsewa anapilila cifukwa anali na “ ciyembekezo cotsimikizika ca zinthu zoyembekezeledwa . ” — Aheb . M’bale Mumba : N’zoona . Conco , pangafunike nthawi ndi khama kufunafuna siketi yosathina , kapena dilesi , bulauzi , suti , kapena thilauzi . Pamene ndinali kusinkhasinkha za citsanzo ca Yesu , ndinazindikila kuti Ufumu wa Mulungu uyenela kukhala cinthu cofunika kwambili m’moyo wanga , m’malo mosakaniza zinthu za ufumu ndi zinthu zina zimene ndinali kukonda . Koma sanali kubeleka . Nthawi ina , iye popemphela anacita lumbilo pamaso pa Yehova kuti ngati adzakhala na mwana wamwamuna , ‘ adzam’peleka kwa Yehova masiku onse a moyo wake . ’ ( 1 Sam . Nawonso anthu amene ali kumbali ya dziko la Satana amakhala na ciyembekezo , koma amakayikila ngati zimene akuyembekezela zingacitike . Pamene tiphunzila za makhalidwe abwino a Yehova , timam’yandikila kwambili . Olo kuti zinali conco , Yehova sanafulumile kuusiya mtundu umenewu . John anaona kuti cimene cingathandize munthu kupilila mavuto ndi kukhala wolimba mwa kuuzimu . Iye “ sanali kusoŵa pakacisi . Anali kucita utumiki wopatulika usana ndi usiku . ” Baibo imati : “ Monga mwa Adamu onse akufa , momwemonso mwa Khristu onse adzapatsidwa moyo . ” ( Yohane 1 : 1 ; Chivumbulutso 3 : 14 ) Mngelo ameneyo ndi Yesu , ndipo Yehova anali kumuuza maganizo ake ndi mmene anali kumvelela . Iwo angalephele kumvetsetsa cifukwa cake Mlengi wacikondi amalola mavuto . N’cifukwa ciani Iye anacita zinthu mwanjila imeneyi ? ’ Adamu atafa sanakhale cinthu cina kapena kukhala ndi moyo kwinakwake . 5 : 25 - 27 ) Motelo , io amakhala oyela . Makolo angasankhe kuti mmodzi wa io aziphunzila mabuku amenewa ndi mwana panthawi ina osati pa kulambila kwa pabanja . Timaŵelenga Baibulo monga banja masiku onse pofuna kuonetsa ciyamikilo cathu kwa Yehova kaamba ka Baibulo limeneli . ” Mauwo anali akuti : ‘ Kilogalamu imodzi ya tiligu , mtengo wake ukhala dinali imodzi , ndipo makilogalamu atatu a balele , mtengo wake ukhala dinali imodzi . Koma musawononge mafuta a maolivi ndi vinyo . ’ ” — Chivumbulutso 6 : 5 , 6 . 5 : 1 - 4 ) Mwacionekele , zimenezi zinasangalatsa kwambili oyang’anila oyendela monga Paulo , pamene anali kucezela mipingo . Koma kumbukilani Mau a Paulo akuti : “ Iye [ Yehova ] adzapeleka njila yopulumukila kuti muthe kuwapilila . ” Mwacitsanzo , kodi mungapeleke ndalama kuti mugule nyumba imene simudziŵa bwino ? Iwo amakamba kuti munthu amalandila moyo wosatha akafa na kuyenda kumwamba . Ndipo n’naona munthu wina woyofya m’maonekedwe akunikonkha , wokhala na zolemba - lemba pakhungu mofanana na anthu amene anali kudana ndi anthu akuda . Kodi “ masiku oipa ” ndi ati ? Kupitila m’makonzedwe amenewa , Mulungu anaonetsa kuti moyo ni wopatulika . Komanso , anaonetsa mmene akulu amatithandizila , na zimene kulapa kweni - kweni kumatanthauza . Kale , anthu ena akafuna kudziŵa zakutsogolo anali kufunsila kwa ansembe ocita mayele amene anali kulosela zakutsogolo . Iwo anali kukamba kuti amauza anthu uthenga wocokela kwa mulungu amene anali kuimila . Ndipo Yobu anali kukhulupilila kuti nthawi ina m’tsogolo , Yehova adzam’kumbukila . Kodi Mboni zimacita ciani kuti gulu likhalebe loyela ? Kucokela kum’mawa kwa Ulaya , ku dela la pakati pa America , mpaka kufika ku Africa , Akristu olimba mtima akhala akucitabe mwambo wokumbukila imfa ya Yesu ngakhale panthawi za nkhondo kapena ziletso . Anthu kuno ku Myanmar ali na umoyo wosalila zambili , koma ni aulemu ndipo amamvetsela mwacidwi uthenga wabwino . Akristu amene anadzozedwa sakaikila ngakhale pang’ono kuti anasankhidwa . Kudzakhala kosavuta kwa mkazi kusangalala ndi mangawa a mucikwati ngati mwamuna wake amamusonyeza cikondi nthawi zonse osati panthawi ya kugonana cabe . Tingaonetsenso cifundo mwa kucitila anthu ena zinthu zabwino . Iye anacita mantha kwambili , ndipo anayankha kuti , “ Ai , sindinaonepo . ” Kodi mau a pa Salimo 122 : 3 , 4 tingawagwilizanitse bwanji ndi anthu a Mulungu lelolino ? M’nkhani ziŵilizi , takambilana mmene mapangano amenewo amagwilizanilana ndi mbali zofunika zokhudza Ufumu . Mwacionekele , mwakumbukila kuti anthu anagwila mau a ulosi wokamba za Mesiya amenewa , pamene Yesu anali kuloŵa mu Yerusalemu pa Nisani 9 atakwela pa bulu . ( Aef . 6 : 4 ) Makolo oopa Mulungu amafuna ana awo kukhala monga Samueli , amene Yehova sanamusiye pamene anali kukula . — 1 Sam . ( Machitidwe 3 : 2 - 7 ; 9 : 36 - 42 ) Mwacitsanzo , io anali kucilitsa anthu ndi kukamba zinenelo zosiyanasiyana . Nkhani yonse ya m’caputala cimeneci itithandiza kudziŵa mboni zimenezi . Mungaone mmene nkhope zawo zionekela zacimwemwe pa jw.org . Mgwilizano umene ulipo pakati pa maganizo na thanzi la munthu . ( b ) Ni mavuto abwanji amene anthu ophunzila cinenelo catsopano amakumana nawo ? Nanga izi zibweletsa mafunso yanji ? PAMENE masiku otsiliza akufika kumapeto , anthu oipa akupitiliza ‘ kuphuka ngati msipu . ’ Kukhala m’dziko loipali ni cinthu covuta kwa mtumiki wa Yehova aliyense . Posakhalitsa , n’nakhala na mimba ndipo n’nabeleka mwana wamwamuna nili na zaka 16 cabe . Ca m’ma 1450 , n’zocitika ziti zimene zinayamba kucepetsako mphamvu za cipembedzo conama pa anthu ? Iwo amafuna kuti aziwakonda na kusunga pamtima zimene amawaphunzitsa kuti ziwapindulitse . “ Kodi Mulungu Sindiye Amamasulila Maloto ? ” Kodi ciyenela kukhala cikondi copanda dyela cimene Baibulo limatiphunzitsa kusonyeza anthu onse ? Munthu wolungama Danieli atakhala m’dzenje la mikango yolusa usiku umodzi , iye anakamba kuti anapulumuka cifukwa ‘ Mulungu anatumiza mngelo wake kudzatseka pakamwa pa mikango . ’ — Danieli 6 : 16 , 22 . Paulo ali m’ndende , anayamba kuganizila zimene zinacitika pa tsikulo . N’nayesa kukamba na anthu akufa , n’nali kupita kumanda pamodzi na anzanga a kusukulu , ndiponso tinali kutamba mafilimu ocititsa mantha . Kodi kucita zinthu modzikweza n’kucita bwanji ? “ Kaŵili - kaŵili ngati munthu ni wosangalala ndiponso wokhutila mu umoyo wake , amadzakhala na thanzi labwino m’tsogolo . ” Kunena zoona , masikuwo akanapanda kufupikitsidwa , palibe amene akanapulumuka . ” Pa tsiku limene Yesu anapeleka cenjezo pa nkhani ya kutha kwa cikondi , anachulanso amene tiyenela kum’konda ngako . Conco anali kukhalila kubisala apolisi ndipo anali kugona m’masitiliti . Amakhalanso ndi moyo wokondweletsa Mulungu ndi kugwila nchito mwakhama yopanga ophunzila . 37 : 3 . 17 Yosefe wa ku Arimateya Analimba Mtima Mwacitsanzo , patangopita zaka ziŵili pambuyo potulutsa Baibulo la Dziko Latsopano Lomasulira Malemba Achigiriki Achikhristu , Baibulo lokonzedwanso lochedwa American Standard Version , linatulutsidwa . Ndipo ngati mufuna kudziŵa zimene mwana wanu akuganiza pa nkhani ina yake , mungam’funse maganizo ake pa nkhaniyo , osati ponena za iye . ( Mat . 6 : 22 ) Yesu anaonetsa kuti anthu amene amafunitsitsa “ kudziunjikila cuma padziko , ” amaononga ubale wao ndi Mulungu . — Mat . Koma nawonso anasintha . Iye anali kudziŵanso Ciheberi cakale cimene Mose ndi aneneli anali kukamba , ndipo zolembedwa zao zinali kuŵelengedwa m’masunagoge mlungu uliwonse . Conco , timamuyamikila ngako Yehova cifukwa cotipatsa “ mtendele wa Mulungu . ” ( 2 Mbiri 10 : 1 ) N’kutheka kuti iye anali na nkhawa kuti sadzakwanitsa kulamulila mofanana ndi Solomo , atate wake amene anali na nzelu zapadela . Koma enawa anamangidwa cifukwa ca kuba . ” Mu caputa 11 ya Aheberi , tipezamo maina 16 a atumiki a Mulungu amene anaseŵenzetsa ufulu wawo mosapitilila malile amene Yehova anaika . Ambili aona kuti kudzicepetsa kumawathandiza kukhululukila ena ndi kuiŵalako zimene awalakwila . N’naganiza zokwatila Gloria , mmodzi wa atsikana aja amene ananiitanila ku phunzilo ya buku . ( Onani palagilafu 12 ) Kudzicepetsa kungatithandize ‘ kupitiliza kugonjetsa coipa mwa kucita cabwino . ’ Koma Mulungu yekha ndiye amakulitsa . ( 1 Akor . Kodi ndi kuyeletsa kotani kumene kunacitika kuyambila 1914 mpaka kuciyambi kwa 1919 ? Mwacitsanzo , Yehova amafuna kuti aliyense wa ife akhale wololela ndiponso woganiza bwino . Cifukwa m’pemphelo lake la payekha , munthu ndi mtima wonse , amalonjeza Yehova kuti adzam’tumikila kwa moyo wake wonse zivute zitani . Tinakondwela kwambili kugwila nchito yomanga ya padziko lonse ( Mateyu 20 : 28 ) Pa tsiku lacitatu , Mulungu anamuukitsa “ monga mzimu ” “ ndi kumulola kuonekela ” kwa ena mwa ophunzila ake . Mwacitsanzo , Mark ndi Claire , amene anakulila ku Wales , anayamba upainiya atatsiliza sukulu . Yehova anatuma “ Mwana wake wobadwa yekha ” padziko lapansi kudzatimasula ku ucimo ndi imfa . — Yoh . 3 : 16 . Cifukwa cina cacikulu cimene timalalikilila uthenga wa Ufumu n’cakuti timakonda Yehova na Yesu ndi mtima wonse . ( Maliko 12 : 30 ; Yoh . Kumbukilani kuti Yesu anakamba kuti : “ Ufumu uliwonse wogawanika umatha . ” — Mat . Iye ananipatsa malangizo na kunifotokozela mfundo zina zothandiza . Popeza kuti anyamata amenewa anakana kugwadila fanolo , io anaponyedwa m’ng’anjo yoyaka moto . ( Mat . 16 : 18 , 19 ) Yesu anacenjeza Yakobo , Yohane , Petulo ndi atumwi ena kuti sayenela kukhala odzikonda kapena kudziona kuti io ndi ofunika kuposa abale ao . — Maliko 10 : 35 - 45 . Ganizilani za alongo amene apilila citsutso ca m’banja kwa zaka . 6 : 13 , 17 , 18 ; 2 Pet . ( Yoh . 5 : 15 - 18 ; 7 : 14 ) Iye mopanda mantha anayeletsa kacisi kaŵili konse mwa kuthamangitsa anthu amene anali kuipitsa nyumba yolambililamo . — Mat . Lemba la Akolose 3 : 13 limati : “ Pitilizani kulolelana ndi kukhululukilana ndi mtima wonse , ngati wina ali ndi cifukwa codandaulila za mnzake . Iye anauza Akhiristu anzake odzozedwa kuti : “ Simulinso anthu osadziŵika kapena alendo m’dziko la eni , koma . . . a m’banja la Mulungu . ” Iye anawonjezela kuti : “ Amene angathe kucita zimenezi acite . ” Mwacionekele zingakuŵaŵeni kwambili . 12 : 13 ) Cina , Davide anapemphela kwa Yehova , kuulula macimo ake , kulapa mocokela pansi pa mtima , ndi kucondelela Yehova kuti am’khululukile . ( Sal . 9 Gulu Lake Ladongosolo Monga mwa Buku la Mau Ake Nkhani ino idzatithandiza kuzindikila masautso amene Satana amabweletsa , ndi mmene tingakonzekelele . Wadela amayesetsa kudziŵa abale onse amene alingalilidwa paudindo , ndipo amaseŵenza nawo mu ulaliki ngati n’kotheka . N’ciani cinathandiza Yesu kukhala wacimwemwe ? Koma Yehova amadziŵa mmene angawathetsele , ndipo angatithandize m’njila imene sitinali kuyembekezela . — Ŵelengani 2 Petulo 2 : 9 . Ndinali ndi mwai wotumikila naye , ndipo pambuyo pake ndinapatsidwa nchito yoyang’anila dipatimenti yomasulila mabuku a zinenelo 10 za kum’maŵa kwa Europe . 1 : 46 - 51 ) Motelo , nafenso tiyenela kuphunzitsa acatsopano kuti azikambilana ndi anthu mwaubwenzi ndi momasuka . 9 Ikani Mtima Wanu pa Cuma Cauzimu ( 2 Petulo 2 : 9 ; 3 : 9 ) Zatithandizanso kuona kuti nchito yolalikila ni yofunika kwambili masiku ano . ( Malaki 3 : 7 ) Maka - maka ngati tikulimbana ndi zofooka zinazake , Yehova amafuna kuti tiziyesetse kukana zoipa . Komabe , nitatsala pang’ono kukwanitsa zaka 12 , n’nakhala wofalitsa Ufumu . Kuyambila nthawiyo , n’nayamba kupita muulaliki mokhazikika . Mukamakambilana mungagwilitsile nchito mfundo zopezeka mu Nsanja ya Olonda ya April 15 , 2012 , tsamba 14 mpaka 16 , ndime 8 mpaka 13 ; ndi buku lakuti : “ Khalanibe M’cikondi ca Mulungu , ” nkhani 16 , ndime 1 mpaka 3 . M’buku la Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu , pa peji 184 , pa bokosi yakuti “ Kuthana Ndi Mavuto Ena , ” muli mfundo zimene zingakuthandizeni kuthetsa vuto limeneli . Koma zimenezi si zoona . Mwakutelo , iye anapatsa ophunzila ake ena okhulupilika mwai wodzalamulila naye monga mafumu mu Ufumu wa Mulungu . — Ŵelengani Luka 22 : 28 - 30 . Kupitila mwa mneneli wake Ezekieli , Yehova analosela kuti anthu adzabwelela ku Dziko Lolonjezedwa ndi kugwilizananso kuti akhale mtundu umodzi . Ponena za ulosi wa m’masiku otsiliza , Yesu anakambanso motsimikiza kuti : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” — Mateyu 24 : 14 . Ndipo ena amapita ku malo osangalalila nthaŵi ya usiku kapena ku malo kumene amasisita thupi n’colinga codzutsa cilakolako ca kugonana . Pangakhalenso cifukwa cina . Palibe ciliconse cimene cionetsa kuti anthu angaleke kukoka fodya . Tingacilikize ulamulilo wa Yehova mwa kukhala na mtima wosagaŵanika ndi kum’tumikila mokhulupilika . Yosefe amachulidwa kotsiliza m’Malemba pamene Yesu anali na zaka 12 . 7 , 8 . ( a ) N’cifukwa ciani tifunika kukhala ogwilizanika ? Iye amasangalala mtumiki wa Mulungu akacita chimo lalikulu . A Yohane : Zimenezi n’zosangalatsa kwambili . Ndipo mumayesetsa kumvetsa zimene mwaphunzilapo zokhudza Yehova ndi Yesu , mmene mungatengele makhalidwe ao , ndi mmene mungathandizile ena . Pa nthawi imeneyo , sitidzalimbana ndi cofooka ciliconse ndipo cidzakhala copepuka kutengela makhalidwe a Yehova . Nthawi zina , abale anzao anali kuwapatsa zofunikila , koma io sanali kukakamiza abale kuti awathandize . ( 1 Akor . ( 1 Tim . 6 : 19 ) Mlongo amene tachula poyamba paja anati : “ Tikamatsatila zimene timakhulupilila , timasangalala kwambili . mungangoyankha kuti : “ N’cifukwa ciani ndifunikila kukhulupilila cisanduliko ? Kunali kosavuta kupeza lemba pogwilitsila nchito codex ( Onani ndime 12 ) Zimene tinaona pa ulendo wacidule umenewo , zinaticititsa kutsimikizila kuti tiyenela kukukila kumeneko . ” M’bale Mumba : Ici n’cifukwa cake Mboni za Yehova zimagwilitsila nchito dzina la Mulungu . Yehova Amapeleka Mphoto kwa Anthu Omufuna - funa na Mtima Wonse , Dec . Iye ananena kuti abale ena a mumpingowo ocokela ku Latin America anali kunena mau oipa okhudza dziko limene iye anabadwila , cikhalidwe ca kwao ngakhalenso nyimbo za m’dzikolo . Nthawi zonse , iye anali kuganizila zolalikila ena uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . Komabe , tsiku lina munthu wina wokhala pafupi na ofesi ya nthambi anatipempha kuti tigule malo ake , cifukwa anali kukukila ku United States . Pamene tinali kuphunzila maulosi a m’Baibo , maganizo anga akuti kulibe Mulungu anayamba kusila . * Mwina angakambitsilane zimene aliyense m’banja angacite kuti athandize makolo . Ana angafunike mwamsanga kupita kukacezela makolo ao okalamba amene anadziphweteka cifukwa cakugwa kapena cifukwa ca mavuto ena aakulu . Kodi zina mwa zolinga zimenezo ndi ziti ? Conco , tingadziŵe bwanji ngati cikhulupililo cathu cayamba kufooka ? Tisanayambe kuphunzila Baibulo , ndinafunsa M’bale Gardner kuti , “ Kodi tiphunzila ciani ? ” Ise tonse tingafunike kudzifufuza moona mtima pa nkhaniyi . Kodi Isaki adzamukonda Rabeka ? N’cifukwa ciani anali kuganiza conco ? Mboni za Yehova zidzakondwa kukuthandizani kuphunzila ndi kugwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo . Ndipo “ cophimba ” cimene caphimba anthu onse cidzacotsedwa kwamuyaya . — Yes . Pokonzanso Baibuloli , a m’Komiti Yomasulila Baibulo anapenda mosamalitsa mafunso masausande ambili ocokela kwa omasulila Abale na alongo ena analimbikitsidwa kupita ku Myanmar ataŵelenga nkhani yokamba za dzikolo , imene inatuluka mu Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2013 . Ku Colombia nakonso pa avaleji , 66 pelesenti ya Mboni ndi alongo ndipo 34 pelesenti ndi abale . Muzikhala nawo pa zocitika za maceza . Imodzi mwa iwo ni Mateyu 6 : 34 imene imati : “ Musamade nkhawa za tsiku lotsatila , cifukwa tsiku lotsatila lidzakhala ndi zodetsa nkhawa zakenso . Akristu ambili amene ali ndi zaka za m’ma 50 kapena kuposelapo akali amphamvu . 23 Acicepele — “ Pitilizani Kukonza Cipulumutso Canu ” N’nayamba khalidwe losamvela nili na zaka 10 cabe . lonjezo limene munacita mutayamba utumiki wanthawi zonse wapadela ? Zimenezi zinathandiza Yobu kukhulupilila kuti Yehova adzacotsa mavuto ake panthawi yoyenela . Ataloŵa m’banja , io anapitiliza kucita upainiya . Kupeza mau amenewo kunali kovuta . 11 : 3 ) Ndiye cifukwa cake anthu ozindikila amaseŵenzetsa kwambili maganizo awo , osati maso na matu cabe yayi . Ophunzila a Yesu akalandila mabuku a Malemba Acigiriki Acikhristu , anali kuwaphatikiza pamodzi na Baibo ya Septuagint ya Malemba Aciheberi na kupanga Baibo ya thunthu imene tili nayo masiku ano . Cifukwa cakuti uci wapacisa umanzuna , ndipo umanunkhila kuposa uci umene wapitidwa mphepo . Ngati mumacita manyazi kukamba na anthu amene simuwadziŵa , mungayambe mwa kucita tunthu tung’ono - tung’ono . Mulungu adzakonza ndi kubwezeletsa zinthu za m’cilengedwe n’colinga cakuti zipitilize kucilikiza zamoyo . Kukhala wodzicepetsa sikutanthauza kukhala ndi maganizo olakwika monga akuti , “ Ndine wacikulile ndipo palibe cimene ndingacite . ” Yehova anapatsanso Adamu na Hava lamulo lina , ndipo anawauzilatu cilango cimene adzalandila ngati sadzamvela . Iye anati : “ Usadye zipatso za mtengo wodziwitsa cabwino ndi coipa . Cifukwa tsiku limene udzadya , udzafa ndithu . ” ( Gen . ( 2 Pet . 3 : 9 ) Conco , pambuyo pa cipanduko , mwamsanga Mulungu anapanga makonzedwe akuti anthu akhalenso pa ubwenzi ndi iye , panthawi imodzi - modzi kusungabe miyezo yake yolungama . Ndipo tidzaona cifunilo ca Mulungu cikucitika mokwanila pamene anthu mabiliyoni adzaukitsidwa ndi kukhala m’paladaiso pa dziko lapansi . Kambili n’nali kulalikila nekha . Koma Yehova amachula dzina nyenyezi iliyonse . Ngakhale zinali conco , iwo anaganiza zobweza ndalamazo kwa mwiniwake . Anavomela kucita zonse zofunikila kwa anthu odziŵika ndi dzina la Mulungu . Capamodzi anafuula kuti : “ Zonse zimene Yehova wanena tidzacita zomwezo . ” ( Eks . Panthawiyo , vuto la kupha mafumu kapena kuwacitila ciwembu linali lofala . Kwa zaka 20 , Aisiraeli ‘ anapondelezedwa kwambili ’ ndi Yabini , mfumu yacikanani . ( 1 Yohane 3 : 22 ) Iye amadziŵa kuti timafuna kupezeka pamisonkhano ndipo amayamikila kuyesayesa kwathu . — Aheberi 6 : 10 . Mukakwanilitsa zolinga zanu , mudzakhala wacimwemwe ndi wokhutila podziŵa kuti mwacita zonse zimene mungathe kuti mulalikile uthenga wabwino . M’Baibulo , mulinso nkhani zina zimene zimaimila zinthu zazikulu zodzacitika mtsogolo . Conco , mungacite bwino kusintha maganizo anu , ndipo mukatelo mudzasangalala kutumikila Mulungu ndi anthu ena . 28 : 8 - 10 ; Luka 24 : 13 - 16;30 - 36 ; Yoh . 20 : 11 - 18 . Masiku ano , tikuona kukwanilitsidwa kwa ulosi wa Danieli umenewu . Iye anali kum’dziŵa bwino Mulungu ndipo anakumana ndi zinthu zimene zinalimbitsa cikhulupililo cake . ( Onani bokosi lakuti , “ Dzina Limene Lili ndi Tanthauzo Kwambili . ” ) Akhristu oona amapewa kupeleka ulemu waconco kwa anthu ena . Yehova amatikonda : Yehova amatikonda cifukwa ndife ana ake . Conco , mukadzalandila thandizo mwanjila zimenezi , mukakumbukile Gwelo la thandizolo ndi kuyamikila Mulungu m’pemphelo . — Sal . Cikondi ndi cimene cinatilimbikitsa kudzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa . Ndithudi ! Kukonda anthu anzathu ni cifukwa cabwino cimene cimatilimbikitsa kupitiliza kulalikila . Tinalembela kalata ku likulu , yopempha kuti atitumize ku dela losoŵa . Sindinawadziŵepo ndipo ndinali kuyewa kukhala nao , makamaka nditadziŵa kuti anyamata ena kusukulu anali ndi atate ao . Mukaphunzila zinthu zabwino m’Baibo , kodi simungauzeko ena ? Cigumula cisanacitike , Satana anasonkhezela ena mwa angelo amenewa kubwela pa dziko lapansi na kuyamba kugonana ndi akazi . Kuti acite izi anali kufunika kulolela kusiya nchito na nyumba yake , ndiponso analibe ufulu wotuluka mu mzindawo mpaka pamene mkulu wa ansembe akafe . * ( Num . Olo Mulungu wanu , Yehova , sangakupulumutseni . ’ ( Luka 11 : 13 ) Susi , amene tam’gwila mau poyamba , anati : “ Nthawi zambili tinali kugwada na kucondelela Yehova kuti atitonthoze . Kodi Yehova amamvela bwanji ngati muyesetsa kucilikiza ulamulilo wake ? Ndiye cifukwa cake kumapeto kwa tsiku la 6 la kulenga , Mulungu “ anaona kuti zonse zimene anapanga zinali zabwino kwambili . ” 28 : 18 , 19 ) Kodi mungatsatile bwanji kaphunzitsidwe ka Yesu ? Nanga n’cifukwa ciani na ise tingakhale na cikhulupililo ngati cimeneci ? Pali malemba ena m’Baibo amene aonetsa kuti atumiki okhulupilika a Yehova akale , anali kukhulupilila kuti m’tsogolo akufa adzauka . Iye anati : “ Mutakhulupilila munaikidwa cidindo ca mzimu woyela wolonjezedwawo , umene ndi cikole ca colowa cathu cam’tsogolo . ” Cocitika cosangalatsa cimeneci cinanikumbutsa kufunika kopitiliza kulalikila , cifukwa sitidziŵa malo kapena nthawi imene coonadi cingazike mizu . Ifenso tikamaganizila madalitso amene iwo anapeza , tidzalimbikitsidwa kuyembekezela Yehova moleza mtima . Kodi mukanayamba kuganiza kuti mwina Mulungu ndi wopanda cilungamo ? Atayenda ulendo wolemetsa wa masiku 8 kudutsa m’cipululu , anafika m’dziko la Sudan . Ndipo ndiziiyendetsa ndine osati inu . ” ( Mat . 5 : 37 ) Ena akavomela ciitano kwa wina , amasintha maganizo akalandila ciitano cina cocokela kwa munthu amene aona kuti ali na zinthu zapamwamba . Mabanja ao ali ndi mavuto aakulu , koma banja lathu lili ndi cimwemwe cacikulu . Estienne anagaŵa Malemba Acikristu Acigiliki , kapena kuti Cipangano Catsopano , kukhalanso m’mavesi kuti zifanane ndi Malemba a m’Cipangano cakale . Mngelo anamuuza kuti : “ Danieli , sunga mauwa mwacinsinsi ndipo utseke ndi kumata bukuli kufikila nthawi yamapeto . ” Ndimakondwela kwambili , ndipo ndimatonthozedwa kaamba ka ciyembekezo coti ndidzaonanso atate wanga panthawi ya ciukililo cimene Mau a Mulungu amalonjeza . — Yohane 5 : 28 , 29 . 68 : 19 . Tikuyembekezela mwacidwi nthawi imeneyo . ( Aheb . 10 : 24 , 25 ) Cinanso , tifunika kuseŵenzetsa ziwiya zonse zimene Mulungu amagwilitsila nchito pogaŵila cakudya cauzimu kwa anthu ake padziko lonse . — Luka 12 : 42 . Iye amandithandiza nthawi zonse . ( Mat . 22 : 39 ) Mwacitsanzo , tsiku lina mlongo wina wa ku Ireland anafika pa Nyumba ya Ufumu misonkhano itangotsala pang’ono kuyamba . BEZALELI ndi Oholiabu anali kudziŵa nchito yomanga . 24 : 37 - 39 ) Kodi anthu ena asokonezeka maganizo cifukwa ca zocita ndi mabodza a Satana ? N’cifukwa ninji Yehova anagwilitsila nchito anthu kulemba Baibulo ? Kucita conco , n’kosagwilizana ndi mmene Yehova amacitila zinthu . “ Ndasunga mosamala mau anu mumtima mwanga . ” — SAL . ( Yohane 14 : 15 ) Tikamapemphela kwa Atate wathu wakumwamba , mau apa Salimo 116 : 1 , 2 adzaticititsa kukhala ndi cidalilo cakuti Yehova amamva mapemphelo athu , ndipo tidzamva monga mmene wamasalimo anamvela . Ndipo pambuyo pa Cigumula , anakhalabe wokhulupilika kwa zaka zina 350 . Komanso , monga mmene Baibo imakambila , ‘ pelekani nchito zanu kwa Yehova , ndipo zolinga zanu ndithu zidzakhazikika . ’ — Miy . N’naphunzilanso kutsuka manu na kusakula tsitsi poseŵenzetsa mendo . Kudzicepetsa na kumvela kunam’thandizanso kuti akhale mphunzitsi wacifundo ndi wokoma mtima . Iye “ analiumba kuti anthu akhalemo . ” 1 : 8 ; Akol . ( Luka 7 : 11 - 17 ; 8 : 41 , 42 , 49 - 55 ) Marita na m’bululu wake Mariya anali kudziŵa kuti Yesu anali kukwanitsa kucilitsa odwala . Pambuyo pophunzila Baibulo kwa zaka zitatu , Kingsley anadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa pa September 6 , 2008 . Koma mabwenzi a Mulungu adzapulumuka monga mmene Nowa ndi banja lake anapulumukila . — Mateyu 24 : 37 - 42 . Monga taonela kale , Yesu anadziyelekezela na mtengo wa mpesa , ndipo ophunzila ake anawayelekezela na nthambi . Anakulila ku dela laconde lochedwa Alaotra Mangoro , kum’maŵa kwa dziko la Madagascar . Pamene anali ndi zaka 90 koma wopanda mwana , kuganizila zinthu zabwino zamtsogolo kunamuthandiza kukhala ndi cikhulupililo . Katherine anati : “ Ndiyamikila kuti cikhumbo canga cofuna kuthandizako munthu kukhala mtumiki wa Yehova cakwanilitsika . ” * Koma kodi nsembe imeneyo anangopatsa mtundu wonse wa anthu kapena imaonetsanso kuti Mulungu amacita cidwi ndi inuyo panokha ? Pakamba kuti : “ Akazi agonjele amuna ao ngati mmene amagonjelela Ambuye , cifukwa mwamuna ndiye mutu wa mkazi wake monganso mmene Khristu alili mutu wa mpingo , pokhala mpulumutsi wa thupilo . ” Mulungu amatiuzanso za maulosi amene anakwanilitsidwa kale . 146 : 3 , 4 . Iwo anali kutsatila mosamalitsa mfundo zina zing’ono - zing’ono za m’Cilamulo . Yesu anati : “ Mumapeleka cakhumi ca timbewu ta minti , dilili , ndi citowe . ” Pambuyo pakuti Aiguputo akanthidwa ndi milili 9 , Farao mwaukali anauza Mose kuti : “ Samala ! Ndisadzakuonenso , cifukwa ndikadzangokuonanso udzafa . ” Cimene cinali kuwalimbikitsa ndi kukumbukila za umoyo wa Aisiraeli pa ulendo wawo m’cipululu . Kutsatila ndandanda imeneyo kungatithandize kusinkhasinkha pa zimene Yesu anacita atatsala pang’ono kuphedwa . Sicinali copepuka kukonzekela na kutambitsa makanema amenewa . Kosi imeneyi limodzi ndi mabuku ogwilitsila nchito pophunzila ndi zaulele . Ngati zinthu zimenezo sizinacitike , ndiye kuti cikhulupililo ca Akristu n’copanda nchito , ndipo ciyembekezo cokhala ndi moyo m’Paladaiso ndi loto cabe . Pamene ma Baibo a m’Cizungu anaculuka , anthu otsutsa anakamba kuti sikunali kofunikila kutulutsa ma Baibo osiyana - siyana m’citundu cimodzi . Koma anayamikilanso kukongola kwina kumene Sara anali nako , kumene kunali kuposa kukongola m’maonekedwe . Tingagwilitsile nchito vidiyo yakuti N’ciani Cimacitika ku Nyumba ya Ufumu ? Nthawi zonse , n’nali kumuŵelengela zofalitsa zatsopano zikalibe kupulintiwa . Izi n’zimene Yesu anali kucita . Kodi Satana angayese bwanji kutiopseza ? Malonjezo onse a Yehova amakwanilitsidwa cifukwa iye akupitilizabe kugwila nchito kuti awakwanilitse . ( Yes . Kodi simukuona kuti anthu kulikonse ni odzikonda , okonda ndalama , odzitukumula komanso onyada ? Pakati pa Aleviwo , panali ena okwana 288 , ‘ ophunzitsidwa kuimbila Yehova , ndipo onse anali akatswili . ’ — 1 Mbiri 23 : 5 ; 25 : 7 . Kucita izi ni njila yabwino yoonetsela kuti ndise “ oceleza . ” — Aroma 12 : 13 . Kodi mufunika kukhala woleza mtima , wokoma mtima , kapena wodziletsa ? Patapita nthawi , kalata inabwela , ndipo anatipatsa utumiki woyendela dela . Ifenso tinacita cimodzi - modzi . Kodi zocitika pa umoyo wa Abulahamu zinam’thandiza bwanji kulimbitsa cikhulupililo cake mwa Yehova ? 14 : 21 ) Kuwonjezela apo , pamene timvela lamulo la Yesu lakuti tizilalikila , timaonetsanso kuti timakonda Mulungu , cifukwa malamulo a Yesu ni ogwilizana ndi cifunilo ca Atate ŵake . ( Mat . 17 : 5 ; Yoh . Sitiona ngati kuti timangotaya nthawi yathu . ” Tikadzicepetsa ndi kupempha citsogozo ca Yehova , tidzapewa kupanga zosankha zimene zingatigwetsele m’mavuto aakulu . Kodi tingatsimikize mtima za ciani ? Ndipo ukacikwanilitsa , umamvela bwino na kudziuza kuti , ‘ Yaa , nacita zimene n’nali kufuna ! M’bale Mumba : Poyamba taŵelenga Yohane 14 : 6 . Dikishonale ina inati : “ Ngakhale kuti zimene zinalembedwa pa gumbwa zikuonetsa njila ya kalembedwe katsopano , zolembazi zinalembedwa molondola kwambili ndipo zionetsa kuti Baibulo ni buku lodalilika . ” ( The Anchor Bible Dictionary ) MAKOPE 237,600,000 Kodi tate wina amene anali atapita kukagwila nchito kwina anacitanji kuti athetse vuto m’banja lake ? Wamasalimo anadziona ngati “ mbalame imene ili yokha - yokha padenga , ” kapena kuti pamtenje . Sakiko anakambanso kuti : “ Tinafunika kucita khama kuti tiphunzile Cipwitikizi , koma madalitso amene tapeza ni oculuka kwambili . Abele ayenela kuti sanali kudziŵa mmene mau amene Mulungu anauza njoka adzakwanilitsidwila . Mulungu anati : “ Ndidzaika cidani pakati pa iwe ndi mkaziyo , ndi pakati pa mbeu yako ndi mbeu yake . Mbeu ya mkaziyo idzaphwanya mutu wako , ndipo iwe udzaivulaza cidendene . ” ( Gen . Cacitatu , Akhristu amene akutumikila Yehova mokhulupilika ngakhale kuti akutsutsidwa , afunika kuyamikilidwa ngako cifukwa ca kukhulupilika kwawo . Mipata ngati iyi ingathandize acinyamata kumasuka ndi kukamba za kukhosi kwao . ( b ) N’cifukwa ciani tinganene kuti anthu ocita zoipa afika poipa kwambili ? 5 : 28 ) Kumbukilani zimene zinacitikila Mfumu Davide . ( Yakobo 4 : 8 ) Conco , kodi tidzapindula bwanji ngati timapemphela tsiku ndi tsiku ? Baibo imakamba kuti : “ Atabatizidwa , nthawi yomweyo Yesu anavuuka m’madzimo . Tikamatelo , Yehova adzasamalila zosoŵa zathu . ( Mat . 12 : 11 ) Conco , mayeselo amenewo sayenela kutilanda cimwemwe . Koma mmene Mose anali kulangizila ndi kutsogolela anthu , zinaonetselatu kuti anali kuthandizidwadi ndi angelo . Komabe , tonse amuna ndi akazi tingaphunzilepo kanthu pa kudzicepetsa kwa Rabeka . Ndani wa ife amene sangafune kukhala ndi khalidwe lofunika limeneli ? Koma cifukwa cakuti sindinawauze zimene anali kufuna , anayamba kundimenya mpaka ndinakomoka . ( Aefeso 4 : 24 ) Tikupemphani kuti mudziŵe zambili zokhudza Mboni za Yehova , zimene zimakhulupilila , ndi mmene zingakuthandizileni kudziŵa zimene Mulungu walonjeza kudzacita m’dziko latsopano . 1 : 9 , 10 ) Ngati mwayamikilidwanso monga mkulu , muziyang’ana kwa Yehova kuti akupatseni mphamvu kuti mukhale odekha ndi acimwemwe . Anakambanso kuti , “ Uzim’kumbukila m’njila zako zonse , ndipo iye adzawongola njila zako . ” ( Miy . Kuitaniwa Kucoka mu Mdima , Nov . Taphunzila kuti tingapindule ndi mbali zonse za Baibulo . Koma Paulo na Sila coyamba anapita kukalaila kwa Lidiya , amene anali atangobatizika kumene . Nthawi zina tikamayesedwa , Yehova angalole mayeselowo kuti tiphunzilepo kanthu kena . ( Aroma 5 : 8 ) Ngati tilapa mocokela pansi pamtima ndi kukhulupilila nsembe ya dipo , Mulungu adzatikhululukila macimo athu . Timayamikila Yehova kwambili pa cikondi cimene anaonetsa potumiza Mwana wake kudzatifela . — Yoh . 3 : 16 . Yohane analemba kuti : “ Mulungu anatisonyeza ife cikondi cake pakuti anatumiza m’dziko Mwana wake wobadwa yekha kuti tipeze moyo kudzela mwa iye . ” ( 1 Yoh . 8 : 9 ) Koma kumaiko ena , ndevu sizololeka kwa Akhiristu . — w16.09 , peji 21 . Saona kuti msonkhano uli pafupi kuyamba . Zaonekelatu kuti sali maso , sadziŵa kuti ni nthawi bwanji , ndipo saona zimene zicitika . M’kupita kwa nthawi , Mfumu Davide analinganiza Alevi ndi ansembe m’magulu awo . Komanso onani citsanzo cina cosonyeza mmene nchito ya Ufumu yapitila patsogolo mocititsa cidwi . Yesu sanauze otsatila ake kuti anyamule malupanga monga zida zodzitetezela . NYIMBO : 87 , 3 Tingadzifunse kuti : ‘ Kodi ndimatumikila Yehova cifukwa com’konda ndi kulemekeza ulamulilo wake ? Ganizilani za Kaini . Rutherford . Sitingafotokoze bwinobwino mmene zinacitikila kuti ana a Adamu ndi mbadwa zake zamtsogolo atengele ucimo umenewo . Kuti tikhale ndi cikhulupililo cotelo , tifunika kuphunzila za Mulungu woona . “ Atate wanu wa kumwamba . . . amawalitsila dzuŵa lake pa anthu oipa ndi abwino , ndi kuvumbitsila mvula anthu olungama ndi osalungama omwe . ” — Mateyu 5 : 45 . ( a ) Ndi mtundu uti wa ulaliki wapoyela umene mumakonda kwambili ? Koma mwacionekele , anaona kuti n’nali kukonda zinthu zauzimu . Kodi lemba la Mika 6 : 8 lingatithandize bwanji kuti mavalidwe athu akhale olemekeza Mulungu ? 20 : 4 - 6 ; 34 : 12 - 16 . Mosiyanako , ise timanyadila kuuza anthu amene amatifunsa kuti mtsogoleli wathu si munthu wopanda ungwilo . ( Aheb . 9 : 6 , 7 , 11 - 14 , 24 - 28 ) Ndife oyamikila kwambili kuti macimo athu amakhululukidwa , ndi kuti tili ndi cikumbumtima coyela cifukwa cokhulupilila nsembe ya Yesu . Ni m’buku la Yohane cabe la Uthenga Wabwino mmene timapezamo mfundo ya Yesu yakuti cikondi ndiye cimadziŵikitsa ophunzila oona a Khristu . — Ŵelengani Yohane 13 : 34 , 35 . Cofunika kwambili ni kuphunzila kuona zinthu mmene Yehova amazionela . Ndipo mtumiki wothandiza akamatumikila modzipeleka , mtsogolo angadzayenelele kukhala mkulu . M’masophenya amenewo , Ezekieli anaona zinthu zambili zoipa zikucitika mumzindawo . 4 : 13 . ( Salimo 33 : 5 ; 37 : 28 ) N’cifukwa cake sangalole anthu ankhanza kukhalapo mpaka kalekale . Ndidzamudalitsa ndipo adzakhala mayi wa mitundu yambili ya anthu ndi wa mafumu a mitundu yambili ya anthu . ” ( Gen . M’Baibulo limenelo , dzina la Mulungu linali kupezeka nthawi zoŵelengeka cabe , ngakhale kuti m’mipukutu yakale limapezeka masauzande ambili . NYIMBO : 34 , 61 ( Oweruza 11 : 36 ) Analola kukhala wosakwatiwa ndiponso kusakhala ndi ana kuti atumikile Yehova . Oyang’anila dela ndi akazi ao amaoneka kuti ndi anthu olimba kuuzimu ndi kuti sangagonje pamayeselo . Ise Akhristu sitili pansi pa Cilamulo ca Mose . Mizindayo inali m’madela osiyana - siyana , ndipo kunali miseu yokonzedwa bwino yopita ku mzinda uliwonse . ( Maliko 7 : 5 , 10 - 13 ) Yesu anapeleka citsanzo cabwino pankhani imeneyi . Panthawi imeneyo , ambili anakhala ampatuko mwa kutsatila ziphunzitso za zipembedzo zonama ndi kukana coonadi . Yehova akanagwilitsila nchito angelo kulemba Baibulo . Mwacionekele , dzina la Mulungu liyenela kupezeka m’Baibulo . Onani nkhani yakuti , “ Kale Lathu — Padutsa Zaka 100 Tsopano ” mu Nsanja ya Olonda ya February 15 , 2014 , masamba 30 - 32 . Usiku wa tsiku lomwelo , ophunzila aŵili aja anabwelelanso ku Yerusalemu . Citani zotsatilazi kuti mudziikile zolinga na kuzikwanilitsa . Kodi n’zotheka kukhala m’cikondi ceniceni ? Ngati tacita ciwelewele , tinganyozetse dzina loyela la Mulungu . Iwo anaona kuti kumvela Yehova ndiye kofunika kwambili . Pamene Aisiraeli anali ku Babulo , kodi anaona kukwanilitsika kwa ulosi uti wa Yesaya ? Cifukwa ca phokoso la anthu komanso vuto lakumva limene iye anali nalo , ndinafunika kukamba mokweza mau pophunzila . Yehova amakukondani ndipo amafuna kukuthandizani . Inde , anali wodzipeleka pothandiza ena . Koma n’zomvetsa cisoni kuti iye “ anadwala n’kumwalila . ” 10 : 9 , 10 ) Palibe munthu angaonetse cikondi cacikulu kuposa cimene Yesu anationetsa . ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Mumacita ciani kuti ana anu azimasuka kulankhula nanu ? Eliya atafika pafupi ndi tauni ya Abele - mehola , anapeza anthu akulima munda waukulu ndi ng’ombe 24 zimene zinali kukoka mapulawo . N’cifukwa ciani buku la m’Baibulo limeneli n’lothandiza kwa anthu a ku Japan ? Ganizilani za Sadirake , Mesake ndi Abedinego , amene anakana kulambila fano loimila boma la Babulo . Anacitadi momwemo . ” Anaikamo zonse zofunikila kuti tikhale na moyo , na kuti tizikhala osangalala . Inde , mwa “ mzimu wabata ndi wofatsa umene uli wamtengo wapatali pamaso pa Mulungu , ” mkazi angakopele mwamuna wake ku cipembedzo coona mom’fika pamtima , kusiyana ndi kumamuuza mosam’pita m’bali ziphunzitso za Cikhiristu . — 1 Pet . Zimenezi zinali zosiyana kwambili ndi anthu ena a m’dzikolo amene anali ogaŵikana cifukwa cosiyana maganizo m’zandale na m’zacipembedzo . Mgwilizano umenewu ndi wapadela kwambili . Ngati munthu wayamba kuyenda njila yolakwika , Yehova amam’langiza kuti : ‘ Bwelela kwa ine ndipo ine ndibwelela kwa iwe . ’ Tsopano nili ndi zaka zoposa 90 ndipo nchito yanga ni kulimbikitsa atumiki a pa Beteli monga m’busa wakuuzimu . Iwo anasinthilatu . Yehova anali atakambilatu kuti : “ Ndidzalola Farao kuumitsa mtima wake , ndipo adzawathamangila . Ndidzapezelapo ulemelelo mwa kugonjetsa Farao ndi magulu ake onse ankhondo , ndipo Aiguputo adzadziŵa kuti ine ndine Yehova . ” ( Eks . NDANI ANGAKHALE ‘ MLENDO M’CIHEMA ’ CA YEHOVA ? Iye anali kuthawa ndipo analema ngako . ( b ) Kodi Akristu ena akumana ndi masinthidwe otani ? * Komabe , mwacidziŵikile iye anatengela dongosolo la cikwati limene Mulungu anakhazikitsa mu Edeni , n’kulipanga monga lamulo loyenela kulitsatila . Wolemba wina anakamba kuti pemphelo lili ngati “ mankhwala . . . amene amathandiza kuti munthu amveleko bwino . ” Kucita izi kunali kutilimbikitsa kwambili . Ndi Maudi a Mulungu ? TSIKU lina usiku , mtumwi Petulo ndi ophunzila ena analimbana ndi mphepo yamkuntho pa Nyanja ya Galileya pofuna kuolokela ku tsidya lina . 119 : 33 ; 143 : 10 ) Munthu wokonda zinthu zauzimu sacita nchito za thupi , koma amayesetsa kukhala na “ makhalidwe amene mzimu woyela ” umabala . ‘ Kukhalabe maso ’ mwauzimu kumatanthauza zambili kuposa kungocita zoyenela . N’cifukwa cake Baibo imatilangiza kuti : “ Monga Yehova anakukhululukilani ndi mtima wonse , inunso teloni . ” — Akol . M’zaka zaposacedwa , masukulu ophunzitsa atumiki a Mulungu asintha kwambili . Kodi anthu okhala ngati mbuzi adzamva bwanji pamene adzadziŵa kuti atsala pang’ono ‘ kuonongedwa kothelatu ’ ? 10 : 4 , 5 ) Koma vuto lalikulu limene lingasokoneze mtendele wathu , lingacokele kwa acibululu osakhulupilila . Kaya mumakonda kupemphela kapena ai , mungadzifunse kuti : ‘ Kodi kupemphela kuli ndi ubwino wanji ? Ngati masiku ano kuli munthu wamtali conco , n’zosadabwitsa kuti Goliyati anali wamtali mamita 2.9 kapena kuposapo . Mwatsoka lanji , patangopita zaka ziŵili n’nadwala matenda aakulu . Conco anatiuza kuti tibwelele kwathu . M’Malemba , mulibe pamene paonetsa kuti Petulo analandidwa udindo uliwonse . 2 : 13 - 17 ) Nyumba za Ufumu nazonso ndi malo olambilila Yehova ndi kuphunzilila mau ake . Musaiŵale kuti uthenga waukulu womwe uli m’fanizo limeneli ndi wakuti : “ Khalani maso . ” Odessa Tuck , amene panthawiyo anali na zaka 18 , atacoka pamsonkhanowo anatsimikiza mtima kukhala wodzipeleka monga Yesaya . Mneneli Zekariya analosela kuti m’nthawi ya mapeto , anthu padziko lonse adzasangalala kutumikila Yehova pamodzi ndi otsalila a odzozedwa . Mulungu anathandizanso Yosefe kudziŵa tanthauzo la loto limeneli . Nimamuyamikila Yehova cifukwa conipatsa mwayi wokhala m’banja logwilizana , ndipo ndine wokondwa . ” Ndine wokondwa kuti n’napita kukatumikila ku malo osoŵa . Akristu odzozedwa akutengedwa kukhala “ ana ” a Yehova . N’cifukwa ciani nthawi zina Yehova sayankha nthawi yomweyo mapemphelo ndi kutipatsa ciliconse cimene tikufuna ? Phunzitsani Ana Anu Kutumikila Yehova Alonso anati : “ Mkazi wanga ni wokondwela kwambili kuona mmene nasinthila . Akulu mumpingo ndi amene ali oyenelela kwambili kutipatsa thandizo . Iye anati : “ Sin’nakhulupilile zimene madokota anakamba . Mwamunayu wakhala akukonzekeletsa mkwatibwi wake mwa ‘ kumuyeletsa pomusambitsa m’madzi a mau a Mulungu . ’ Kupita patsogolo kwa nchito imeneyi ndi umboni wakuti mapeto ali pafupi . mu Nsanja ya Olonda , ya April 15 ndi ya December 15 , 2009 . Kuganizila citsanzo ca Yosefe kungatithandize kudziŵa zimene tiyenela kucita ngati ena atikhumudwitsa . Anacita kumwetulila . Posacedwapa , m’bale Paul , wacinyamata , ni amene anatenga malo ake . Iye anaseŵenza ndi m’bale Paul kwa zaka zambili . Kukumbukila zimenezi kudzatithandiza kuwamvetsetsa anthu amene angatilankhule mau oipa . 15 : 16 - 21 ) Ndiponso , kunyada kunacititsa Sauli kuganizila kwambili za kudzipangila dzina m’malo mokondweletsa Mulungu . ( 1 Sam . Cifukwa cosankhana mitundu , anthu amacita ciwawa , nkhondo ndiponso amaphana mwacisawawa . Ni mapindu abwanji amene tingapeze ngati tili na cikhulupililo colimba ? Kodi zozizwitsa zimene Yesu anacita zimaonetsa kuti zinthu zidzakhala bwanji m’dziko la tsopano ? Iye anati : “ Yehova amene anandilanditsa m’kamwa mwa mkango ndi m’kamwa mwa cimbalangondo andilanditsanso m’manja mwa Mfilisiti ameneyu . ” Kodi mzimu wa Yehova unatimasula ku zinthu ziti ? Ndipo mfundo imeneyi imakhala yomveka tikaona mmene dziko linalengedwela . Monga mmene tidzaonela , cikondi n’cofunika ngako kuti munthu akhale wacimwemwe . Mu 1950 , n’nasamukila ku Vancouver . Nthawi imeneyo , mkuluyo anapeleka uphungu kwa m’baleyo . ( Mac . 1 : 8 ) Kodi akanaigwila bwanji nchito imeneyo ? ( b ) N’ciani cina cimene analamulidwa kucita ? Ndipo n’cifukwa ciani malangizo amenewo amagwilanso nchito kwa makolo masiku ano ? Nimalalikilabe m’njila zosiyana - siyana , monga pafoni na ulaliki wa mwamwayi . Monga taonela , panthawi yovuta ndi ya ciyeso , m’pamene cikhulupililo na kulimba mtima kwake zinali kukulila - kulila . Yesu anaphunzitsa otsatila ake kupempha Yehova kuti awapatse mzimu woyela . Koma iye anazindikila kuti Aroni sanali munthu woipa . 12 : 11 ; 20 : 23 - 27 ) Yehova anayang’ana cikhulupililo ndi kulapa kwa Aroni . Conco , cikondi cathu sicifunika ‘ kukhala caciphamaso , ’ koma cifunika kukhala “ copanda cinyengo . ” Yesu anawauza kuti : “ Munalanda anthu kiyi yowathandiza kudziŵa zinthu . Mutu wa mkazi ndi mwamuna , ndipo mutu wa Kristu ndiye Mulungu . ” Conco , angacite bwino kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ine nimalimbikitsa abale na alongo kukhalabe okhulupilika ? ( Chiv . 2 : 13 ) Iwo anali kuyembekezela mphoto yaciukililo ca moyo wakumwamba . Kwa zaka zambili , naona kuti ceni - ceni cimene cimacititsa anthu kusankhana si kusiyana kwa khungu ayi . Koma ucimo wocokela kwa Adamu , umene tonsefe tinatengela . Tsiku lina mu August 1974 , iye anabwela ku nyumba ya mlongosi wanga , ndipo kumeneko n’kumene tinakumana . ( a ) N’kuti kumene tingapeze zitsanzo za anthu odziletsa ? ( Mat . 24 : 42 ; 25 : 13 ; 26 : 41 ) Izi zionetsa kuti ngati timaona kuti “ cisautso cacikulu ” cikali kutali , kapena kuti cidzabwela ise titafa kale , tingayambe kugwila nchito yathu yolalikila mwamphwayi . ( Mat . Patapita zaka , mtumwi Paulo anafotokoza njila imene iye ndi anzake anapemphelela . Si atumiki onse a Yehova amene akumana ndi mazunzo oopsa . Cifundo ndi khalidwe limene limasonkhezela munthu kuthandiza ena kuti akhale ndi umoyo wabwino . Kupatulapo mtima wofuna udindo ndi ulamulilo , panalinso zinthu zina zimene zikanasokoneza mgwilizano wa ophunzila a Khristu . Koma pofika kumapeto kwa caka cimeneco , amishonale 13 anatumizidwa kumeneko . CIFUKWA CAKE ENA AMAKAIKILA : Anthu ambili amaganiza kuti Mulungu amangowaona monga anthu ocimwa , odetsedwa ndi osafunikila kuwaŵelengela . N’zolimbikitsa kwambili kuti khalidwe la kuzindikila la Yesu linam’cititsa kuonetsa cifundo mwanjila imeneyo . Kodi mungamve bwanji ngati mwalandila mphatso yotelo ? Dzina limene Mulungu anapatsa mwanayo lakuti Isaki , limatanthauza “ Kuseka . ” Kamvedwe kakale : Kopolo woipa ndi waulesi amaimila odzozedwa a m’zaka za m’ma 1914 amene anali kukana kulalikila . Nkhanza ili ngati matenda oopsa amene akufalikila pa dziko lonse . Tidzakambitsilana njila zisanu ziti zoonetsa kuti Mulungu amatiyang’ana cifukwa cotikonda ? Dziŵani kuti “ mutacita cifunilo ca Mulungu , [ mudzalandila ] zimene Mulungu walonjeza . ” ( Aheb . Ngakhale pamene anthu atikwiila ndi kukana uthenga wathu , timaonetsa kuti timakonda anzathu ndipo timatengela citsanzo ca Yesu . Pamene mkazi wanu wadwala , muonetseni kuti mumam’ganizila ndipo khalani woleza mtima . ( b ) Kodi Davide anali kukhulupilila kuti Yehova amucitila ciani ? ( a ) Ndi macenjela akabisila ena ati a Satana ? Citsanzo 2 : Ngati munthu wacipembedzo kwambili amavutika kukhulupilila kuti anthu oipa sadzazunzika kwamuyaya m’moto wa helo . Nchito ya Mboni za Yehova inaletsedwa , ndipo boma linalanda ofesi ya nthambi Ndikuwafuna . Koma nthawi zokwanila 7 zitatha , Nebukadinezara anacila misala yake ndi kuyambanso kulamulila . Munthu wauzimu sagwilizana ndi anthu amene angaike moyo wake wauzimu paciopsezo . M’MAIKO ambili , anthu amaika makamela m’masitolo ao kuti aziona makasitomala ndi kugwila amene akuba zinthu m’sitolo . Kodi khalidwe lanu limaonetsa kuti ndinudi Mboni ya Yehova ? Mofanana ndi Yesu , tingapange zosankha zabwino ngati timadalila Yehova . 24 : 6 . Zocitikazi zimakhudza moyo wathu masiku ano ndiponso tsogolo lathu . Nthawi zambili , zimene Baibo imakamba ponena za mbalame za m’mlenga - lenga , zimatiphunzitsa mfundo zofunika pa umoyo ndi pa ubwenzi wathu na Mulungu . Anthu ambili mumzindawo akucita mantha kwambili . Banja limeneli linayamba nchito ya ukopotala , ndipo mwana wao wamkazi , Yukiko , anapita kukatumikila pa Beteli ku Tokyo . Yesu atafa , Petulo anabwelela ku nchito yake yakale ya usodzi . Zinthu zoipa zimene ndinaona zinandikhudza kwambili . N’cifukwa ninji mabuku athu akhala akufotokoza kuti mwina Yesu anali kukamba za ciukililo ca padziko lapansi ? ( Ŵelengani Yakobo 3 : 9 , 10 . ) Ng’ombe zonenepazo ndi ngala 7 zooneka bwino zinali kuimila zaka 7 zimene zinali kudzakhala ndi cakudya cambili . Koma ng’ombe zowonda ndi ngala zopanda kanthu zinali kuimila zaka 7 za njala zimene zinali kudzabwela pambuyo pa zaka za cakudya cambili . Nthawi ina capakati pa March ndi April anapita kukacezela anzao amene anali kukhala kudela la West Coast ku United States . ( 1 Mbiri 29 : 5 ) Mukanakhalapo , kodi mukanayankha bwanji ? Tiyeni tione zimene iye anakamba pa Yohane 14 : 1 . Baruki anamvela malangizo a Yehova ndipo anapulumutsa moyo wake . — Yeremiya 45 : 2 - 5 . Banjalo linafuna kupatsa Haykanush ndalama pofuna kumuyamikila , koma iye anakana . 1 , 2 . ( a ) N’ciani cionetsa kuti mpingo wa m’nthawi ya atumwi ku Kolose unali pa mavuto ? M’madela a mapili a kumeneko , tinapeza anthu ambili odzicepetsa okamba Ciudu , amene anali na njala ya coonadi . Koma tingafunse kuti : Kodi Yehova wakhala bwanji Mfumu masiku ano ? Yesu anauza ophunzila ake kupemphela kuti ufumuwo ubwele , cifukwa udzabwezeletsa cilungamo ndi mtendele padziko lapansi . Mbali imeneyo ilinso ndi malo amene mungalembepo zolinga zimene mufuna kukwanilitsa pa nkhani ya pemphelo , phunzilo laumwini , ndi polalikila . Mwacitsanzo , taganizani mmene tinali kufotokozela fanizo la Yesu lokhudza Msamariya wacifundo . Mosiyana na Yehova na Yesu , akulu sangaone za mumtima mwa munthu . Anafuna kuphunzila zambili koma anali kucita mantha ndi zimene ena angakambe akamuona akukamba ndi Yesu . Tingathandizile motani pa nchito yofunika ya Yehova ? Pamene dziko la Poland linabwezeletsa ufulu wake pambuyo pa Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse , anthu m’dzikolo anaculuka kwambili . Mzimayi uja ataona mayankhidwe ofatsa a Toñi , anagwetsa misozi . ( 1 Pet . 2 : 22 ) Ubatizo wake unali umboni wakuti wadzipeleka kuti acite cifunilo ca Mulungu . — Aheb . Patapita zaka ziŵili , ndinauzidwa kuti ndizitumikila monga mpainiya wapadela . Pamene mukuyenda , mwaloŵa m’ngalande yaitali imene muli mdima . Ana ndi akulu omwe , anali kungondiyang’ana , kundilondola ndi kundiseka . Anthu ena amene timaphunzila nao Baibulo ndiponso amene akhala akusonkhana nafe kwa nthawi yaitali , amazengeleza kubatizidwa . Buku la Mau a Yehova limalangiza ise tonse kumvela na kugonjela . Conco , anatumiza munthu amene anaonetsa bwino makhalidwe ndi umunthu wa Yehova . A Zimba : Koma tidziŵa bwanji zimenezo ? ZIMENE MUNGACITE KUTI MUTHANDIZE ENA N’cifukwa ciani Akristu amene atumikila zaka zambili ndi ofunika ? Kodi Abulahamu anacitanji ? M’nkhani ino , tidzakambilana mafunso atatu ofunika kwambili . M’bale Gardner anandiuza mokoma mtima kuti , “ Cabwino , tiye tikambilane mutu woyamba . ” Koma sitiyenela kunyodola ena , kuwacititsa manyazi , kapena kuwatukwana pofuna kuseketsa anzathu . Baibo imati : “ Mulungu akuonetsa cikondi cake kwa ife , moti pamene tinali ocimwa , Khristu anatifela . ” Ngakhale kuti sanadziŵe zonse zokhudza kukwanilitsidwa kwa malonjezo a Mulungu , cikhulupililo cinam’thandiza kuona mphoto yosaoneka . Komabe comvetsa cisoni n’cakuti io anataya ubwenzi wao ndi Mulungu . Nayenso anali kulakwitsa monga mmene ife timacitila . Iwo anacimwa kwambili cakuti Yehova anawalanga mwa kulola kuti Ababulo awatenge ndi kupita nawo kwawo monga akapolo . ( Yes . Ndinakondwela kudziŵa kuti Mulungu ali ndi dzina , lakuti Yehova , ndipo linali kuchulidwa kaŵilikaŵili . Atumiki ambili a Mulungu masiku ano sadzapita kumwamba . Ganizilaninso za Yosefe , mwana wa Yakobo . Ndiponso mtumwi Petulo anakana Yesu . “ Tiyeni tilimbikitsane , ndipo tiwonjezele kucita zimenezi , makamaka pamene mukuona kuti tsikulo likuyandikila . ” — AHEB . Kutsogoleledwa ndi Yehova , ndiponso kukhala m’cikondi cake cosatha ndi cinthu cabwino kwambili kuposa cina ciliconse . 16 , 17 . ( a ) N’cifukwa ciani tifunika kudziŵa maganizo a Yehova tisanapange zosankha ? N’zokondweletsa kuti zocitika za pa lemba la Chivumbulutso 11 : 1 , 2 zimagwilizana ndi nthawi pamene kacisi wa kuuzimu anali kudzayezedwa , kapena kupimidwa . Ponena za mauwo a pa Aroma 8 : 5 , katswili wina anati : “ Anthu a conco amasumika maganizo awo pa zinthu za thupi , kumacita nazo cidwi kwambili , kuzikambapo - kambapo nthawi zonse , ndi kuzikhumbila . ” Patapita masiku atatu , Yehova anamuukitsa monga mzimu kuti m’kupita kwa nthawi adzapite kumwamba . ( Levitiko 19 : 15 ) Mulimonse mmene zinalili , oweluza anali kufunika kuweluza mwacilungamo , osati kuweluza mogwilizana ndi maonekedwe a munthu kapena kuchuka kwake . Fotokozani zitsanzo zoonetsa mmene khalidwe la tsankho lingatikhudzile . 11 : 11 , 12 . DEBORA akuyang’ana asilikali amene asonkhana pamwamba pa Phili la Tabori . ( Gen . 12 : 10 - 20 ; 14 : 8 - 16 ; 16 : 4 , 5 ; 20 : 1 - 18 ; 21 : 8 , 9 ) Ngakhale zinali conco , Abulahamu anakhalabe na cimwemwe mumtima mwake . ( Salimo 27 : 10 ) Iye amatikonda kwambili ndi kutisamalila m’njila zambili . Mwacitsanzo , ŵelengani nkhani yakuti “ Kodi Mungakatumikire Kumene Kukufunika Ofalitsa Ufumu Ambiri ? ” ndi yakuti “ Kodi Mungawolokere ku Makedoniya ? ” N’ciani cingawononge unansi wathu ndi Yehova ? Bukuli limakamba kuti Paulo anali ‘ wamfupi , wadazi , wamatewe , woumbika bwino , wa nsidze zambili , ndi wa mphuno yotalikilapo . ’ ” Iye afunika kupumula . Anthu mamiliyoni amayankha kuti , “ Inde . ” Kupemphela pamodzi tsiku ndi tsiku n’kofunika kwambili kuti banja lizikaniza misampha ya Satana . Aliyense wokhulupilila mwa ine , ngakhale amwalile , adzakhalanso ndi moyo . ” — Yohane 11 : 25 . Nchito yolalikila ya padziko lonse itapita patsogolo , panafunika amishonali . M’Baibo mulinso zitsanzo za anthu amene anakhalabe acimwemwe olo kuti anakumana na mavuto . Abulahamu ni mmodzi mwa iwo . Ndinatsatila malangizo opezeka pa Miyambo 13 : 20 akuti : “ Munthu woyenda ndi anthu anzelu adzakhala wanzelu , koma wocita zinthu ndi anthu opusa adzapeza mavuto . ” Tiyeni tikambilane njila zinayi zimene tingacitile zimenezi . Yoyamba ni pemphelo locokela pansi pamtima , ina ni kuŵelenga Mau a Mulungu na kuwasinkha - sinkha , inanso ni kupempha mzimu woyela wa Yehova , komanso ina ni kuuzako munthu amene mumam’dalila nkhawa zanu . Kuti afike ku Kanani , io anayenda mtunda wa makilomita 1,600 . ( 1 Samueli 3 : 10 - 14 ) Mukanakhalapo m’nthawi ya Eli ndi kumuona akulekelela ana ake kucita zinthu zonyansa , kodi sembe munakhumudwa ? Nanga tingatsimikize bwanji kuti Yehova adzateteza gulu lake pa cisautso cacikulu cimene cayandikila ? Cotelo , sitiyenela kupewa cabe kucita ciwelewele koma tiyenelanso kupewa maganizo ndi zilakolako zoipa zimene zingaticititse ciwelewele . — Mateyu 5 : 27 , 28 . Iwo anakambilana ndi mlongo wina amene anali kutumikila ku malo osoŵa ku Ghana ndi kumufunsa mafunso ambili . Pezani malo abata . N’naona monga Tsiku la Ciweluzo lafika , ndi kuti siningapulumuke cifukwa n’nali wosakonzeka . ” — Crystal . Coyamba , ena a ife tinaphunzila coonadi kucokela kwa Akhristu okhulupilika amene anadzipeleka kuyenda mtunda utali kuti akatiphunzitse . Pambuyo pake , bungwelo limapeleka cigamulo pa mfundozo . Ndiyeno , abalewa amaonetsetsa kuti zimene zagamulidwa zacitika . Ngati timamvela malamulo olungama a Yehova na mfundo zake , timaonetsa kuti timam’dalila ndiponso timafuna kukhala naye pa ubwenzi wolimba . ( Yer . 17 : 7 , 8 ; Yak . Tikamacita zimenezi , ndiye kuti ndise omvela . N’zomvetsa cisoni kuti ukapolo ukupitilizabe ngakhale masiku ano . 20 : 2 , 3 ) Yehova sanalole kuti wopha mnzakeyo adzapatsiwenso cilango mtsogolo cifukwa ca chimo lakelo . Pamene ife Mboni tinali kutulutsidwa m’ndende kuciyambi kwa caka ca 1951 , nayenso anatulutsidwa . Muzithandiza ena kulimbitsa cikhulupililo cao . Conco , tikamatumikila Yehova , timakhala na umoyo wacimwemwe kwambili . Yesu anapulumuka pa cocitika coopsaco . Koma kodi izi zikusonyeza ciani ponena za mdani wathu Satana ? Inu acinyamata amene munaleledwa ndi makolo amene ndi a Mboni za Yehova , muyenela kukhala osamala kwambili kuti musataye colowa cakuuzimu cimene munalandila . ( Mat . Iye anali pamalilo a atate ake amene anafa pangozi ya galimoto . Timaikanso zabwino za anzathu patsogolo pa zathu , timakhalanso osamala ndi kupeza zolakwa zikulu - zikulu . 11 : 26 ) Pa lembali , mau akuti “ adzafike ” akamba za nthawi ya ‘ kubwela ’ kwa Yesu , kumene iye anakamba mu ulosi wake wonena za mapeto a nthawi ino . Miyambo 24 : 10 imati : “ Ukafooka pa tsiku la masautso , mphamvu zako zidzakhala zocepa . ” Tonse tingavomeleze kuti zimatenga nthawi kuti munthu acile matenda aakulu . Jacqueline anasangalala cifukwa cotsatila zimene cikumbumtima cake cophunzitsidwa bwino cinamuuza . Tonsefe timaganizila za mtsogolo . Coyamba , sitiyenela kudabwa na mavuto aconco , cifukwa Satana ali pa nkhondo na ise . Conco , inu alonda musaŵavutitse mwa kuŵapempha fodya kapena kuŵatuma kuti akakutengeleni nkhuni yamoto kuti muyatsile fodya . Kodi “ dziko ” limene “ likupita ” liphatikizapo ciani ? Kukamba zoona , kupemphela kumathandiza kwambili . ” Kodi mumasamalila banja ? 3 : 1 - 4 ) Conco , zinthu zimene mtumwi Paulo anaona m’masomphenya ake zinayamba kukwanilitsidwa . Popeza anthu a ku Tuvalu amakonda kuŵelenga , io anasangalala kwambili ndi kutulutsidwa kwa mabuku ndi magazini amenewo . 22 : 19 - 21 ) Izi zinacitika pa nthawi imene Mfumu Senakeribu ya Asuri anali kufuna kuwononga Yerusalemu . Anthu a Mulungu ndi ogwilizana : Kulikonse kumene timakhala , timalambila Yehova ndi kumvela Mtsogoleli wathu , Yesu . 9 : 1 , 11 ; 20 : 1 - 3 ) Tiyeni tipende mmene lemba la Salimo 45 linaloselela zocitika zocititsa cidwi zimenezi . Pang’ono m’pang’ono , timayamba kudziŵa zimene Khristu angacite pa cocitika ciliconse . Tonsefe tili na mwayi wogwila nawo nchito yaikulu yophunzitsa anthu , imene Yehova afuna kuti icitike masiku ano . M’dziko la Satanali anthu ambili ndi okhulupilika ku dziko lao , fuko lao , ndi cikhalidwe cao . ( b ) Mumadziŵa bwanji kuti Satana aliko ? Kumafuna khama na kudzimana . Mofananamo , sitingaononge nthawi yathu kuganizila za ciyembezedzo cimene si ceniceni kwa ife . ( Afil . 3 : 16 ) Pofuna kutithandiza kuti tipitilizebe kupita patsogolo mwauzimu , tidzayankha mafunso atatu m’nkhani ino , ( 1 ) Tingadzipende bwanji kuti tidziŵe ngati ndife ofikapo mwauzimu ? Onse mwamuna na mkazi afunika kucitila zinthu pamodzi kuti banja lawo liyende bwino . ” — Christopher . Aisiraeli atayamba kukhala m’Dziko Lolonjezedwa , anafunika kupanga cosankha cofunika kwambili . Anafunika kusankha kutumikila Yehova kapena kutumikila mulungu wina ( kapena milungu ina ) . Kodi mgwilizano wathu umakopa bwanji anthu kuti aphunzile coonadi ? 1 - 3 . ( a ) N’ciani cionetsa kuti maganizo ndiponso mau a Mulungu ndi apamwamba kuposa a anthu ? Kodi ungaliphunzile bwanji lemba la Genesis 3 : 15 ? Ndipo milandu 24 tinapambanila mu Khoti Loona za Ufulu wa Anthu ku Ulaya . Paulo anati : “ Pamaso pa Mulungu , takhala citsanzo cabwino kwa cikumbumtima ca munthu aliyense . ” — 2 Akorinto 4 : 2 . Munthu wakale Elihu anati : “ Masiku alankhule . Zaka zambili n’zimene ziyenela kudziŵitsa anthu nzelu . ” Munjila ina tingati ndi kusadzikonda . Inde , Yesu ndi mbali yoyamba ya mbeu ya Abulahamu , amene ‘ adzaononga nchito za Mdyelekezi . ’ ( 1 Yoh . Pakati pao pali alongo oposa 50 amene ndi mbeta . Munthu wina amene kale sanali kukhulupilila Mulungu anati : “ Cilengedwe cinandithandiza kukhulupilila kuti Mulungu amafuna kuti anthu azisangalala ndi moyo , conco sadzalola kuti mavuto apitilize kwamuyaya . Cacitatu , mufunika kukulitsa cikondi codzimana , cimene n’cizindikilo ca Akhristu oona . ( Yoh . Luigi anangolemba dzina la kampani ya inshuwalansi ya motoka ya munthuyo , n’kumusiya akali kukalipa . Conco , mwamsanga anatula pansi mtsuko ndi kupatsa mwamunayo madzi kuti amwe . 23 : 15 ) Ndipo Yehova amawadziwa bwino anthu amene amam’tumikila na mtima wonse moti amalemba maina awo ‘ m’buku la cikumbutso . ’ Kumatanthauza kucitapo kanthu . Cikhulupililo cathu mu dipo cimaonekela mwa nchito zathu . M’malamulo 10 , Yehova anapeleka lamulo lakuti anthu ake sayenela kulambila milungu ina . Lembali limati : “ Iwowa adzamenyana ndi Mwanawankhosa , koma pakuti iye ndiye Mbuye wa ambuye ndi Mfumu ya mafumu , Mwanawankhosayo adzawagonjetsa . Ndipo n’cifukwa ciani afunika kulemekezedwa ? 3 Anadzipeleka na Mtima Wonse — ku Madagascar Maganizo aconco amaonetsa mzimu wa dziko , osati nzelu yocokela kumwamba . N’zoona kuti zosankha zimenezi n’zofunika kwambili . Koma , mungacite bwino coyamba kusankha kutumikila Yehova ndi mtima wonse . ( Deut . Komanso , ganizilani za akulu amene amagwila nchito yofunika kwambili m’Makomiti Okambilana ndi Acipatala . Anthu ambili amapeza cimwemwe akakwanilitsa colinga cawo , kapena akagula cinthu cimene anali kufuna . Amai anali kucilikiza atate akamacita mwambo wosala kudya m’mwezi wa Ramadan . Naonso atate anali kucilikiza amai akamacita mwambo wa Pasika . ( b ) Nanga mapemphelo anu angaphunzitse bwanji ana anu kudalila Mulungu ? Citsanzo coyamba ndi cokhudza mfundo ina ya mu Utumiki wa Ufumu pa mbali zoyambitsa maphunzilo a Baibulo . Koma n’zomvetsa cisoni kuti ambili sanayambe kufunafuna cuma cakuuzimu cimeneci . TSAMBA 12 • NYIMBO : 135 , 133 TIMAPEZA madalitso ambili cifukwa ca nsembe ya dipo la Yesu Khiristu . Kodi kuukitsidwa kwa Yesu kusiyana bwanji na kwa anthu amene anaukitsidwa iye asanabwele padziko ? Afunikanso kukhala okondana mofikapo , cakuti ni ofunitsitsa kudzipeleka kwa wina na mnzake kuti amange banja . Iye anakamba nkhaniyi pafupi - fupi ola limodzi na hafu . Mau ake amphamvu anali kumveka m’holo yonseyo pamene anali kufotokoza mmene aneneli akale analengezela mopanda mantha za Ufumu umene ukubwelawo . Kapolo ameneyu amapeleka cakudya cabwino cakuuzimu nthawi zonse kwa anthu onse amene ali mu “ gulu limodzi ” limene Yesu akuyang’anila . ( Mat . Yesu popita kukapemphela , anauza Petulo , Yakobo , ndi Yohane kuti ‘ akhalebe maso . ’ Iye angatiyese mwa kutiwopseza , ndipo imeneyi ni “ imodzi mwa njila zakale kwambili zosoceletsela anthu . ” Pamene m’bale woimila likulu lathu anacezela abale ndi alongo ndi kuwafunsa mmene zinthu zilili , io anati : “ Zonse zili bwino , Yehova anatithandiza . ” Ayi ndithu . Iye sanacilitse khate cabe , koma anacilitsanso matenda amtundu uliwonse ndi zofooka zilizonse za anthu . Koma musanacite izi , seŵenzetsani mwaluso zofalitsa zokhala na malangizo othandizila acicepele , zimene gulu la Yehova lapeleka kwa makolo . Kenneth , amene anapuma pa nchito yake yomanga , ndi mkazi wake Maureen , a zaka za m’ma 50 anasamukila ku California kuti akathandize kumanga likulu ku Warwick . ( Ekisodo 20 : 7 ) Kumakhala kulakwa ngati tiseŵenzetsa dzina la Mulungu mopanda ulemu . — Yeremiya 29 : 9 . Ngati pacitika zinthu zimene zingasokoneze ubwenzi wanu , n’ciani cingakuthandizeni kuupulumutsa ? Iwo aona cizindikilo ca kukhalapo kwa Yesu , ndipo akudziŵa kuti iye akulamulila monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu . 13 : 22 ) Gawo lalikulu la moyo wake , Davide anali munthu wokhulupilika . Ŵelengani Aroma 8 : 4 - 13 . Filimu inayake yoopsa yaposacedwapa inali ndi mutu wakuti Wokana Kristu . Onani kuti uthengawo unali wamphamvu kwambili . Mau akuti “ anthu osaopa Mulungu , ” anachulidwa kanayi pofuna kudzudzula anthu ndi nchito zawo zoipa . Anali okhulupilika kwa Iye ndi mtima wonse . — Danieli 2 : 1 – 3 : 30 . Kudziŵa ciyambi cake kungakuthandizeni kuwayelekezela bwino . Nthawi zina , popeleka moni timacita kugwilana kumanja kapena kugwada . Ma Baibo a m’Cilatini analiko osiyana - siyana . Nanga n’cifukwa ciani panafunika ina yatsopano ? N’cimodzi - modzinso na mkazi wosakhulupilila . Iye afunika kuonetsedwa cikondi ceni - ceni na mwamuna wake wacikhristu . — Aef . Ana anu angaphunzile zambili m’mapemphelo amene mumapeleka . Ganizilani zimene munthu wina analemba zokhudza amayi ake acikulile , amene anali kudwala matenda a mu ubongo . 1 : 8 ) Ndipo anawalonjezanso kuti iye adzawacilikiza panchito yofunika imeneyo mpaka masiku athu ano . — Mat . “ Ofalitsa Ufumu ku Britain — Galamukani ! ” N’cifukwa ciani Akhristu acicepele afunika kukhala olimba mtima ? Musacite manyazi kupempha ena kuti akuthandizeni kudziŵa moseŵenzetsela bwino zida zimenezi . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Mwamunanso asasiye mkazi wake . ” — 1 Akorinto 7 : 11 . Mu 1947 Mboni za Yehova zambili zinabwelela ku Poland zitapemphedwa ndi boma . Nthawi zina ndikaganizila za thanzi langa tsopano , ndimakhumudwa ndipo ndimalila . Olo kuti Timoteyo anabadwila m’banja la makolo osiyana zikhulupililo , amayi ake aciyuda ndi ambuye ake aakazi anam’thandiza kumvetsetsa Malemba , mogwilizana ndi cidziŵitso cimene Ayuda anali naco pa nthawiyo . Iye amacita zosemphana ndi nzelu zonse zopindulitsa . ” Lamulo la Yesu lakuti olambila oona adzalambila Mulungu motsogoleledwa ndi mzimu ndi coonadi , limaonetselatu kuti kulambila mu tuakacisi kapena pa malo opatulika sikukondweletsa Atate wathu wakumwamba . Ngati makolo apempha thandizo kwa Akhristu ena , sindiye kuti akupatsa ena udindo wawo wophunzitsa ana . Koma kucita zimenezi kungakhale mbali yolelela ana awo “ m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake . ” Kunabwela makina atsopano osindikizila amene athandiza kuti mabuku ambili azipulintidwa panthawi imodzi ndiponso azioneka okongola . Tikakumana na vuto , tinali kuŵelenga pa Yesaya 41 : 10 , pamene Yehova anati : “ Usacite mantha , pakuti ndili nawe . Koma n’zosavuta munthu kudziŵa zoona pankhaniyi . * Kukhulupilika kwanu potumikila Yehova kumalimbikitsa ambili , ngakhale aciyambakale m’coonadi . Koma zinthu zinasintha n’taphunzila za ciukililo cimene Yesu anali kuphunzitsa . Zolengedwazo zimafuula kuti : “ Ndinu woyenela , inu Yehova Mulungu wathu wamphamvu , kulandila ulemelelo ndi ulemu , cifukwa munalenga zinthu zonse , ndipo mwa kufuna kwanu , zinakhalapo ndipo zinalengedwa . ” — Chiv . Zithunzi za Paulo zimene zimapezeka m’zofalitsa zathu n’zongoyelekezela cabe , ndipo si zozikidwa pa umboni wodalilika wa zinthu zakale . 4 : 22 - 24 ) M’nkhani ino tikambilana mfundo zimene zingatithandize kuthetsa khalidwe la tsankho . Kupeleka cuma cathu kwa iye ni umboni wakuti timam’konda na kuti timayamikila zonse zimene waticitila . Kodi tiyenela kucita ciani kuti Yehova aticitile cifundo na kutikhululukila ? Iwo amatumikila Yehova m’bwalo la padziko lapansi la kacisi wauzimu . — Chiv . Ndiye cifukwa cake tiyenela kuŵelenga Mau a Mulungu tsiku lililonse ndi kuganizila zimene Yehova amatiuza . Akangofika pa Beteli , io angayambe kuyewa kunyumba cifukwa cokhala kutali ndi banja lao ndi mabwenzi . Limodzi la maiko amenewo linali America . Kumeneko , Charles Taze Russell na anzake oŵelengeka anayamba kuphunzila Baibo mwakhama . Izi zinacitika mu 1870 . Nanga ndi anthu ati amene tingakhale nao paubwenzi ? Ophunzilawo afunika kucita khama kufufuza m’Malemba kuti apeze nzelu zamtengo wapatali . 1 : 7 . Kum’langa mwa njila imeneyo kunam’thandiza kwambili . Ndikumbukila bwinobwino mmene Mboni zinali kuonekela zokoma mtima ndi zacilungamo pa nkhope zao . Ca kumapeto kwa 1989 , ulamulilo wa cikomunizimu wa kum’maŵa kwa Europe usanagwe , Bungwe Lolamulila linatipempha kuti tisamukile ku likulu ku New York . ( Yakobo 1 : 23 - 25 ) Pamene mucita zimenezi , mudzaona kuti malangizo ake ni othandiza . Iwo sangakonde kulandila mauthenga ambilimbili okhudza nkhani zoseketsa , mavidiyo , ndi zithunzi . Ndinauza wolemba nchito kuti ndifuna kusintha umoyo wanga ndi kuti ndizigwila nchito yabwino . Ndiponso ena anali m’zipani zandale , anali abusa acipembezo , ndipo ena anali ofunitsitsa nchito zapamwamba kwambili . Davide anafika mpaka potuma Uliya kukapeleka kalata yokhala na malangizo amene anacititsa kuti Uliyayo aphedwe . ( 2 Sam . ( Mac . 14 : 19 - 22 ) Mwacitsanzo , m’zaka za m’ma 1930 mpaka kuciyambi kwa zaka za m’ma 1940 , abale athu ku United States anakumana ndi citsutso coopsa . Kaya tili pa banja kapena ai , Nyimbo ya Solomo ingatithandize kudziŵa cikondi ceniceni ndi mmene tingacisonyezele . Nthawi yeniyeni imene Yehova anakhazikitsa pangano ndi Abulahamu sidziŵika . Anthuwo anaphunzila kuti pali Mulungu mmodzi woona , ndi kuti amene amam’tumikila ayenela kutsatila mfundo zake za makhalidwe abwino . 1 : 10 ) Ndipo sitimakondwela ngati ndandanda yathu yasokonezeka . Tsanzilani Cikhulupililo Cao — Anapilila Zinthu Zopanda Cilungamo 28 Munthu wakupha mnzake mwangozi anayenela kucitapo kanthu kuti acitilidwe cifundo . Malemba amati : “ Pamene io anali kuvutika m’masautso ao onse , iyenso anali kuvutika . ” Davideyo ndiye anali kudzakhala mfumu yotsatila ya Isiraeli . Ndipo “ akulu , ” amene anali kulemekezedwa cifukwa ca nzelu zao , anaikidwa kukhala oweluza . ( Deut . 25 : 7 , 8 ) Cilamulo cinali kutsogolela mtundu watsopano umenewu pankhani ya kulambila ndi pa zocita zao . Simuyenela kuganiza kuti muyenela kupeza nchito coyamba kuti mudzatumikile Yehova mtsogolo . Mosakaikila , katundu wawo wambili anafunika kuugulitsa kapena kupatsa ena . Nthawi idzafika pamene “ Adamu womalizila ” adzapatsa “ mzimu wopatsa moyo ” kwa anthu onse . Pambuyo pocezela aneneli a ku Yeriko , Eliya ndi Elisa anapita kumtsinje wa Yorodano . Onani kabokosi kakuti “ Kadzioneleni Mwekha ! ” ” Yosefe sanali mtumiki woyamba kapena womaliza wa Yehova kuuzidwa kuti apeleke uthenga wa ulosi umene sudzasangalatsa anthu ndipo udzamubweletsela cizunzo . Komabe amakhala ndi cimwemwe cacikulu kwambili akamalalikila uthenga wa Ufumu kwa anthu amene amaulandila . A Zulu : Musade nkhawa . Ndiye cifukwa cake kaŵili - kaŵili atumwi m’makalata awo , anali kuchula Akhristu anzawo kuti ‘ abale na alongo . ’ — Aroma 1 : 13 ; 1 Pet . Tili ndi moyo , nzelu , thanzi ndi zinthu zocilikiza moyo . Muyenela kudziŵa kuti zakudya zimene anali kudya kwao n’zosiyana ndi zimene inu mumadya . Iwo anati : “ Tikuyamikila kwambili Yehova ndiponso kapolo wokhulupilika ndi wanzelu potipatsa Baibulo limeneli . 19 : 35 - 41 ) Pambuyo pake , Paulo ali ku Kaisareya , anapempha kuti agwilitsile nchito ufulu wake mwa kukaonekela kwa mfumu ya Aroma . Ndipo Yesu anakamba kuti nthawi idzafika pamene “ onse ali m’manda acikumbutso adzatuluka . ” — Yohane 5 : 28 , 29 . Conco , pamene tigwila nchito yathu yolalikila , anthu afunika kukhudzika mtima ndi zimene timawaphunzitsa kucokela m’Baibulo . Koma kenako akunenanso kuti : “ Makiyi sindikupatsani . Kukamba zoona , kukoma mtima kosatha kwa Yehova kumaticititsa kukhala naye paubwenzi wolimba . Kuti nyumba zimenezi zimangidwe , pakufunikila anchito ambili odzipeleka amene ali ndi maluso apadela . Kumbukilani za mwamuna uja wa ciwelewele ku Korinto . Iye anakonda zinthu za “ thupi ” cakuti anafika pocotsedwa mumpingo . Izi zanithandiza kukhala munthu wocezeka , ndipo tsopano nili na anzanga ambili . ” N’ciani cinathandiza Abulahamu kukhala ndi cikhulupililo colimba ? Ndithudi ! Iye ni Tate wanga weni - weni . Kumapeto kwa kalatayo , bungwe lolamulila linalemba kuti : “ Mukamapewa zinthu zimenezi mosamala kwambili , zinthu zidzakuyendelani bwino . Ngati pali cinthu cimene Lefèvre anali kulakalaka pa umoyo wake wonse , ni kuona anthu akusiya miyambo ya anthu ndi kuyamba kucita zinthu mogwilizana ndi cidziŵitso colongosoka ca m’Malemba . Olamulila anzake amenewa adzakhala pambali pake pamene Yesu adzacita “ zinthu zocititsa mantha ” ndi kulamulila mitundu ya anthu ndi ndodo yacitsulo . MFUMU IPAMBANA PA NKHONDO YAKE M’fanizo la anamwali , Yesu anagogomezela mfundo yakuti odzozedwa ake onse ayenela kukhala okonzeka komanso kukhala maso podziŵa kuti Yesu adzabwela pa tsiku kapena ola limene sakuyembekezela . Kukonda zinthu zosangalatsa kunawapangitsa kukhala odzikonda . Mwacitsanzo , polenga zinthu iye anagwila nchito ndi Mwana wake woyamba kubadwa . Komabe pali mabanja ena amene amasamukila kudziko lina kaamba ka zinthu za kuuzimu mofanana ndi mmene Abrahamu ndi Sara anacitila . ( Gen . Vesiyi imalonjeza kuti “ cilengedweco cidzamasulidwa ku ukapolo wa kuvunda n’kukhala ndi ufulu waulemelelo wa ana a Mulungu . ” 3 , 4 . ( a ) Ndi anthu ati amene anaukitsidwa atumwi a Yesu anasabadwe ? Zimenezi zinanipatsa mwayi wokwanilitsa colinga cina cauzimu . Iwo sadzakhalakonso . — Sal . Munthu woyamba kufa anali Abele wokhulupilika . Mwacitsanzo , m’malo mouza anthu kuti kulosela n’koipa , mosadziŵa tinali kuwauza kuti afunika kupewa kugwilitsila nchito masikelo opimila zinthu ndi ndodo zoyendela . 20 : 28 . 7 , 8 . ( a ) N’ciani cingakhumudwitse makolo pambuyo pobwelela kunyumba ? “ Nthawi zonse mau anu azikhala acisomo , . . . kuti mudziŵe mmene mungayankhile wina aliyense . ” — AKOL . ( b ) N’ciani cingatithandize kuti tikhalebe odzicepetsa ? Ufumu wa Mulungu ukadzabwela udzayeletsa dzina lake , ndipo anthu onse adzayamba kulambila Yehova mogwilizana . Mumtima , ndimangoti Mulungu sangandikhululukile . Mkaziyo anafika pamene panali Yesu ndi kugwila ulusi wopota wa m’mphepete mwa covala cake ndipo nthawi yomweyo anacila . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . ” — Chivumbulutso 21 : 4 . Mwa mau ouzilidwa a Petulo amenewa , Yehova amatsimikizila atumiki ake kuti adzawalimbitsa na kuwapatsa mphamvu . Motelo , Yesu anayamikila Mariya cifukwa comvetsela bwinobwino kwa iye . M’nthawi ya atumwi , Akristu ambili anali kulalikila mwakhama ngakhale kuti ambili a io anali kukhalabe kumadela ao ndipo sanali amishonale . N’zolimbikitsa kudziŵa kuti lonjezo lakuti akufa adzauka lingakwanilitsidwe ngakhale patapita zaka zambili . Iye anati : “ Cikondi n’coleza mtima ndiponso n’cokoma mtima . Kodi tingaonetse bwanji mzimu wodzimana ? Nanga kuonetsa mtima umenewu n’kofunika bwanji ? Ambili amakopeka na khalidwe lake labwino . ( Yohane 6 : 44 ) Iye anali kudziŵa kuti muli ndi zofooka ndipo nthawi zina mudzalakwitsa . ( Ŵelengani Aroma 13 : 11 ) Tikukhala m’nyengo imeneyo , imene ndi masiku otsiliza . 4 : 16 - 18 ; Aheb . 6 : 18 , 19 ) Nanga n’ciani cingathandizenso amene asamalila okalamba ? Poyamba iye anali yekha na Yehova . ( Miy . Mulungu amafuna kuti tim’peze . 14 : 16 , 17 . Iye anapita kukafunsila za nkhaniyi kwa mkulu wina , ndipo mkuluyo anamuuza kuti asanapange cosankha , aganizile zotulukapo zoipa zimene zingabwele , monga kutengela mzimu wa mpikisano . ( Onani ndime 16 ) Nthawi zina , tingafunike kuganizilaponso pa cosankha cimene tinapanga . Ndipo dziŵani kuti ngati mugwila nawo mokwanila nchito yolalikila “ mpaka kumalekezelo a dziko lapansi , ” mudzalandila madalitso osaneneka . — Mac . Mwina Mateyu yemweyo ndi amene analimasulila . Onani Buku la Anthu Onse , tsamba 7 - 9 , pa mutu wakuti “ Kodi Bukulo Linapulumuka Bwanji ? ” Conco , n’napita kunyumba kwawo , ndipo tinakambilana kwa nthawi yaitali mocita kulembelana . ( Ŵelengani Yeremiya 10 : 23 . ) Kodi Abulahamu anavutika cifukwa copatsa Loti malo abwino ? Pamapeto pake , apolisi ananigwila , ndipo n’nakhala m’ndende zaka zinayi . Nanga bwanji acibululu ? Koma Yehova anamupatsa mphamvu , ndipo inenso amanilimbikitsa . Mwacibadwa , mbalame zimafunitsitsa kuteteza ana awo . Kuti mudziŵe zambili zokhudza angelo , onani nkhani 10 m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , komanso zakumapeto pa mutu wakuti “ Kodi Mikayeli Mkulu wa Angelo Ndani ? ” Iye anamvela Mulungu ndi kusiya cuma cake ndi umoyo wabwino mumzinda wa Uri ndi kukhala m’mahema kwa zaka zambili . “ MUNTHU ameneyu ndi ciwiya canga cocita kusankhidwa cotengela dzina langa kupita nalo kwa anthu a mitundu ina , komanso kwa mafumu . ” ( Mac . Conco , muziwagwilitsila nchito cifukwa angakuthandizeni kukhalabe acangu ndi acimwemwe mu utumiki . Rahabi ( Aroma 12 : 15 ) Nafenso tiyenela kucita cimodzimodzi . Iwo sanalingane na Mulungu monga mmene Satana anakambila . 12 : 20 ) Kodi mauwa akutanthauza ciani ? Yesu sanali kuvutitsa anthu kapena kuwazunza . Koma anali kuwalimbikitsa ndi mau ake . Kulalikila kumatithandizanso kukhalabe ndi makhalidwe abwino amene amatiteteza kwa Satana ndi dziko lake . — Ŵelengani Aefeso 6 : 14 - 17 . ( 2 Pet . 2 : 5 ) Panthawi ina , Mulungu analamula Abulahamu kuti apeleke mwana wake Isaki nsembe . Akristu onse ndi okondwela kudziŵa za cikwati cochulidwa m’fanizo la Yesu . N’zoonekelatu kuti panthawi yovuta imeneyo , m’bale Russell anali kugwilitsidwa nchito ndi Yehova komanso mutu wa mpingo . Khalani ndi zolinga zauzimu Popeza mngelo ameneyu akamba kuti ‘ opani Mulungu , ’ kodi muganiza kuti akamba za Mulungu uti ? Cifukwa ca mmene mwamunayo anali kumuyang’anila , Rabeka anayesetsa kukhala woolowa manja mmene angathele . ( Ŵelengani Mateyu 23 : 11 , 12 . ) “ Cifukwa ca kudzipeleka mwaufulu kwa anthu , tamandani Yehova . ” — OWER . Mwacitsanzo , Yosefe , Mose , ndi Davide anakumana ndi mavuto aakulu . Tinakwatilana mu December 1971 , ndipo ndikuyamikila kuti kucokela nthawiyo , Susan wakhala akundithandiza nthawi zonse . Zofalitsa zathu zambili amalembela Mboni za Yehova zonse . Mu 1947 , n’nabwelela ku Karachi kuti nikasakile nchito . Kodi anthu amene anafa posacedwa ndiwo adzayambile kuuka mu Ulamulilo wa Khristu wa Zaka 1,000 , kuti akalandilidwe na okondedwa awo amene akuwadziŵa ? 11 , 12 . ( a ) Kodi Hezekiya anaonetsa bwanji za mumtima mwake ? M’bale wina anali kutipatsa ndalama zolipilila zinthu zina . Pamene mulalikila uthenga wabwino , mumathandiza kukwanilitsa ulosi umenewo . ​ — Mateyu 28 : ​ 19 , 20 . Kenako , Koresi anamasula Ayuda ndi kuwauza kuti akamangenso kacisi wao ku Yerusalemu . Komabe , tikaona mbili ya Mabaibo amenewa na ena amene afalitsidwa , timapeza umboni wakuti lonjezo la Yehova lakwanilitsidwa , lakuti Mau ake adzakhala mpaka kale - kale . Palibe nthawi yoikika ya kutalika kwa phunzilo , zimadalila mmene inuyo mwalinganizila zinthu . Ngakhale n’conco , Yesu anapeleka moyo wake kutipulumutsa ku ucimo ndi imfa . — Ŵelengani Mateyu 20 : 28 ; Aroma 6 : 23 . N’cifukwa ciani Marita anali kukhulupilila zimenezi ? Iwo anacitadi zimenezo . — Mat . Kodi mumakamba mau monga akuti , “ Nidzakusiya ine ” kapena “ Nidzapeza wina amene anganikonde ” ? 7 : 32 - 35 . Kodi tiphunzilapo ciani pa citsanzo ca Yehova ? Nkhani iliyonse imene tinali kuphunzila , ndinali kupeza mayankho okhutilitsa a m’Baibulo pa mafunso anga . Mocenjela Yosefe anati kwa abale ake : “ Mvelani maloto amene ine ndinalota . ” Umakhala wokonzeka kukhululuka komanso kupepesa ukalakwitsa . Yesu anafotokoza mfundo imene imatithandiza kudziŵa amene tiyenela kumvela . Ngati mutengela cikhulupililo ndi kumvela kwa Nowa , Yehova sadzalephela kukusamalilani . — Afil . Popeza kuti Yehova wationetsa kukoma mtima kwake kwakukulu , tiyeni tizicita zilizonse zimene tingathe kuti ‘ ticitile umboni mokwanila za uthenga wabwino wa kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . ’ ( Mac . Timakhala pa unansi wabwino na Mulungu . ( 2 Tim . 3 : 1 , 3 ) Popeza kuti anthu ambili m’dzikoli ni osagwilizana , kodi Akhristu angateteze bwanji mgwilizano wawo ? Mwina anacita cidwi poona kuti agaluwo sanatilume kapenanso cifukwa cakuti tinalimba mtima pamene tinawopsezedwa na agaluwo . Mau otsatila amene Zekariya anakamba , anathandiza kuti Ayudawo asakhalenso amantha kapena okayikila . Nanga ife tikadzakalamba , n’ndani adzatisamalila ? Munda umenewo unali wa Naboti , koma Ahabu anali kuusilila . Iwo amadziŵa kuti “ kapolo wa Ambuye sayenela kukangana ndi anthu , koma ayenela kukhala wodekha kwa onse . ” — 2 Tim . 41 : 10 , 13 ) Khalani osangalala podziŵa kuti Yehova na Yesu amakondwela namwe , ndipo adzakudalitsani cifukwa ca kukhulupilika kwanu . Mau awo amanilimbikitsa kwambili ! ” Tsiku lina atakolewa , anapha cisumbali cake ndipo anaweluzidwa kuti akakhale m’ndende kwa zaka 20 . Mboni za Yehova zimadziŵika cifukwa ca nchito yolalikila kunyumba ndi nyumba ndi m’miseu , ndipo nthawi zina zimagwilitsila nchito matebulo ndi mashelufu amawilo oikapo mabuku ndi magazini . Nkhaniyi idzafotokoza malangizo abwino amene tikawaseŵenzetsa angatithandize kuonetsa kuwala kwathu mokwanila . Mtima wa Mkhristu ni mbali yofunika ngako . N’cifukwa cake timauzidwa kuti tizikonda Yehova ndi mtima wathu wonse ndi kukonda anzathu mmene timadzikondela tokha . ( Miy . 3 : 11 , 12 ) Apa pali phunzilo lofunika ngako kwa Akhristu amene anacotsedwa pa udindo mu mpingo , kapena amene alandiwa mwayi wa utumiki wina wake . Cina , malangizo amene timalandila pamisonkhano amalimbitsa cikhulupililo cathu . Anakwanitsa kumanga bwino cingalawa olo kuti kunali kuyamba . Mwacitsanzo , pamene Mkulu wa Ansembe Kayafa anakamba kuti , “ Ndikukulumbilitsa pali Mulungu wamoyo , utiuze ngati ndiwedi Khiristu Mwana wa Mulungu ! ” Yesu anakamba moona mtima ndipo anamuuza kuti ndine Mesiya . Patapita nthawi , Hezekiya anadwala mpaka kutsala pang’ono kufa . Baibulo limatiuza kuti pemphelo limakhudza mbali zonse za umoyo wathu . Mwacionekele , iye anakwiya poona kupanda cilungamo kumene anthuwo anaonetsa pobwela kudzagwila Yesu usiku . Nayenso Jae - won wa zaka 76 wa ku South Korea amayamikila abale amene amamunyamula pa galimoto kupita ku Nyumba ya Ufumu . Mofananamo , sitingayembekezele kuti anthu ambili adzabwela m’gulu la Yehova panthawi yocepa yabata imeneyo mkati mwa cisautso cacikulu . Citsanzo ca Yesu citiphunzitsa kuti tifunika kukhala okhulupilika kwa Yehova ndi kwa anthu ake . M’pamene n’namvetsetsa nkhani za m’Baibulo zimene n’naphunzila pamene n’nali mwana kwambili . Ndiyeno anaonjezela kuti : ‘ Ana a Isiraeli ukawauze kuti “ Ndidzakhala Amene Ndidzafuna Kukhala ndiye wandituma kwa inu . ” ’ ” ( Eks . Matthew Kodi cilango ca Mulungu cimatikonzekeletsa ciani ? ( Luka 10 : 21 ) Pa cocitika cina , “ Yesu anakweza maso ake kumwamba ndi kunena kuti : ‘ Atate , ndikukuyamikilani kuti mwandimva . ’ ” ( Akuluwo anali kuyamikila kwambili utumiki wa amishonalewo ndipo anati adzapeleka thandizo lonse lofunikila kwa makolowo . Anakwanitsa kucita zimenezi cifukwa cakuti alonda amene anali pa mageti a mzindawo anali m’tulo . Ataloŵa mkacisi , anauwocha ndi kuwononga mzinda wonse wa Yerusalemu . Dzipeleke pa zinthu zimenezi kuti anthu onse aone kuti ukupita patsogolo . ” — 1 TIMOTEYO 4 : 15 . Timaonetsanso kuyamikila kuti Yehova amatikhululukila . — Akol . Conco , ngati mwininyumba amakaikila zakuti Mulungu aliko , tingam’funse kuti , “ Kodi amenewo ndiwo maganizo anu kuyambila kale ? ” Pa cisautso cacikulu , iye adzaika cizindikilo a khamu lalikulu pamene adzawaweluza kuti ni nkhosa . Kumbukilani kuti mzimu wa Mulungu ndiwo umakolezela cimwemwe . Hiroo wakhala zaka 12 ku Russia tsopano ndipo watumikila m’mipingo yosiyanasiyana . M’malo mwake , iye atafa anakhala wopanda moyo monga fumbi limene anamuumbila . — Genesis 2 : 7 ; Mlaliki 9 : 5 , 10 . Koma Baibulo limatsimikizila kuti Mulungu , Mlengi wathu , sadzalola anthu kuononga cilengedwe kothelatu . Komabe , Akhiristu ambili amatengela Yesu . Alendo amenewo ayenela kuti anali amishonale , nthumwi za Yohane , kapena oyang’anila oyendela . Iye anati : “ ‘ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi maganizo ako onse . ’ Mau amenewa anali aulemu m’nthawi za m’Baibo . Mofanana ndi zimene Petulo anacita pambuyo pokumana ndi Yesu , nafenso tifunika kuonetsa kuti timakondadi Khristu mwa kuika patsogolo nchito imene watipatsa . A munthu aliyense Koma ngakhale tiyese bwanji , sitingadziŵe caka , kapena tsiku ndi ola limene cisautso cacikulu cidzayamba . Mgwilizano umenewo wakhalapo cifukwa ca “ cilankhulo coyela , ” cimene ndi miyezo ya Mulungu yolambilila . — Zefaniya 3 : 9 ; Yesaya 2 : 2 - 4 . N’cifukwa ciani timapewa kukamba bodza ? Zimene Yehova amalonjeza adzakwanilitsadi . Ndiyeno , mungaŵalongoze webusaiti ya jw.org na kuwaonetsa mavidiyo na zofalitsa zimene zilipo m’citundu cawo . — Deut . 1 , 2 . ( a ) Kodi makolo ena acikhristu amamvela bwanji mwana wawo akawauza kuti afuna kubatizika ? 6 , 7 . ( a ) Kodi mtima wonyenga ungapangitse munthu kucita ciani ? Nanga bwanji za kuukila mwakabisila ? Atakambilana nkhani zambili za m’Baibulo anaonanso kuti Jairo akumvetsa kufunika kokhala Mkristu wobatizidwa . 3 : 17 - 20 ) * Iwo anafunikila kucita zinthu monga akazembe m’malo mwa Kristu . Unali wotambulula , cakuti munthu angathe kuuŵelenga . ( Yohane 13 : 34 , 35 ) M’kupita kwa nthawi , ine ndi Laurie tinabatizidwa kukhala a Mboni za Yehova . Mlongo wina ku Australia anakhudzidwa kwambili na mmene wokamba nkhani wina anafotokozela malemba pamsonkhano wampingo . Koma , namonso mulibiletu caka cimeneci . Koma kenako , a David anayamba kuŵelenga magazini amene Mary anali kuwapatsa . Ganizilani cabe mmene dziko likanaipila ngati aliyense analibe cikumbumtima . Panayiota anati : “ Pamisonkhano imeneyi , ndinaona anthu akuonetsana cikondi ceniceni , cimene sindinacionepo zaka zonse zimene ndinali kucita zandale . ” Anthu ambili amakamba kuti sitingadziŵe za kumwamba cifukwa kulibe aliyense wocokela kumwamba amene anabwela padziko lapansi kudzatiuza mmene kulili . Paulo anadzipeleka ngako kulalikila mumzinda umenewo , ndipo anali kukonda “ oyela ” anzake . ( 1 Akor . Inakambanso kuti anthu adzakhala osadziletsa , na oopsa . Conco , Langton anagawanso Baibulo kuti likhale ndi macaputala . Zili na matupi ang’ono koma zimadya kambili patsiku kuposa munthu . Iwo safanana cifukwa amacokela ku maiko osiyanasiyana , anakulila ku malo osiyanasiyana , ndi a msinkhu wosiyana , ndipo amakonda zinthu zosiyana . Onani zitsanzo izi : “ Khamu lalikulu ” la anthu ocokela m’mitundu yonse lidzapulumuka “ cisautso cacikulu , ” cimene cidzathetsedwa pa nkhondo ya Aramagedo . — Chivumbulutso 7 : 9 , 14 . Zimenezo zandipatsako mphamvu . Cikwati cinatha ndi mkazi wanga ndipo n’nayamba kukumana ndi mavuto ambili . Atanena mau amenewa , Amai anayamba kulila . Mwacidule , tiyeni tikambilane zimene Paulo anakamba ponena za cikondi , ndipo tidzaonanso mmene mau ake angatithandizile pocita zinthu ndi anzathu . 16 : 15 ) Tiyeni titumikile Yehova modzipeleka tili ndi cidalilo cakuti iye ‘ amathandiza anthu amene amamuyembekezela ’ — Yes . ( 1 Atesalonika 5 : 12 ) Ndipo ngati tiwalemekeza kwambili , m’pamenenso amasangalala kwambili ndi utumiki wao . — Aheberi 13 : 17 . Ndiye cifukwa cake Akatolika ambili amakhulupilila kuti kuloŵana m’malo kwa atumwi ndi ciphunzitso cofunika kwambili . Conco , ziphunzitso zonse za Akatolika , kaya n’zoona kapena ai zimadalila pa ciphunzitso cimeneci . Komabe , Yehova analola kuti Yesu aphedwe ndi adani ake . Mwadyela io anali kufuna zambili . Ali na zaka za m’ma 60 , anali atatumikila monga mmishonale ku Ivory Coast ( Lomba lochedwa Côte d’Ivoire ) kwa zaka 20 . Pasanapite nthawi , aŵiliwa anayamba kucita umishonale pamodzi . — Mac . 13 : 2 , 3 . 2 : 6 ) Yesu anakhala nsembe ya dipo imene inatsegula njila ya ku moyo wosatha kwa “ anthu ambili ” — amuna , akazi , ndi ana . ( Mat . Zimene zinayambitsa kucepako mphamvu kwa Babulu Wamkulu pa akapolo ake ni kubwela kwa mashini opulinthila mabuku , ndi anthu olimba mtima omasulila Baibo ( Onani palagilafu 12 na 13 ) Kodi uphungu wa Yesu unali kunena za nthawi iti ? M’machechi yambili mwamuna kapena mkazi amakhala mtsogoleli kapena m’busa . M’zaka za m’mbuyomu , zofalitsa zathu zakhala zikufotokoza tanthauzo la dzina la Mulungu mwa kugwilitsila nchito lemba la Ekisodo 3 : 14 , limene limati : “ Ndidzakhala Amene Ndidzafuna Kukhala . ” ( Gen . 21 : 14 - 21 ; 22 : 2 ) Komanso monga mmene takambila , udindo wokhala woyamba kubadwa unacotsedwa kwa Rubeni n’kupelekedwa kwa Yosefe . Ndithudi , tingagwilitsile nchito Baibulo kudziŵa ngati tili m’cikhulupililo ndi kuona ngati tili wofunika kwa Yehova . Paulo anauza Akhiristu a ku Efeso kuti : “ Munamva kuti ndinaikidwa kukhala woyang’anila kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu kuti ndikuthandizeni . ” Masiku ano , anthu amakwanitsa kuona nyenyezi zambili - mbili kuposa kale . Ndipo izi n’zimene zinapangitsa kuti , kwa nthawi yoyamba , nisiye zinthu zina kuti nikwanilitse zolinga zanga zauzimu . Pamene n’nali ku London , n’nakumana na M’bale Albert Schroeder . Yakobo mwacibadwa anali kudela nkhaŵa ana ake ndiye cifukwa cake anatumiza Yosefe kuti akaŵaone mmene alili . N’cifukwa ciani kukambilana za khalidwe la cifundo n’kofunika ? Ponena za nzelu za Yehova , wophunzila Yakobo analemba kuti , “ coyamba , ndi yoyela , kenako yamtendele , yololela , yokonzeka kumvela , yodzaza ndi cifundo ndi zipatso zabwino , yopanda tsankho , ndiponso yopanda cinyengo . ” Kuonjezela pa Sukulu ya Ulaliki , palinso masukulu ena ophunzitsa Baibo amene akonzedwa kuti aphunzitse akulu mumpingo , apainiya , abale osakwatila , Akristu apabanja , a m’Komiti ya Nthambi ndi akazi ao , oyang’anila oyendela ndi akazi ao ndiponso amishonale . Kodi masomphenya amene Yohane anaona akuonetsa ciani ? Kodi panali ubale wanji pakati pa iye na Yesu ? ( Miy . 5 : 15 - 20 ) Kunena zoona , okwatilana ayenela kusonyezana cikondi ca mitundu yonseyi . ( Pitani pa malo ofufuzila zinthu a pa intaneti ndi kulemba mutu wa kavidiyo kameneka ) Kodi Yehova waonetsa bwanji cikondi cake ? Mwacitsanzo , nimakamba zinthu zabwino zimene utumiki wathu umakwanilitsa ngakhale kuti anthu ena salabadila . ” Panali adani amphamvu ambili a uthenga wa ufumu , koma Yesu anali kufunitsitsa kudziŵa kuti ophunzilawo adzakwanitsa bwanji kugwila nchitoyo . Tiphunzilapo ciani pa citsanzo ca mtumwi Paulo pankhani yokhala woyamikila ? Ife atumiki a Mulungu , tiyenela kuikako nzelu ku umoyo wathu wauzimu na wa banja lathu . ( Mat . A Daka : Mukunena zoona . ( Miyambo 15 : 1 ) Mwacitsanzo , mnyamata wina amene anali kuleledwa ndi amai ake a Mboni anali kucita zoipa kwinaku akutumikila Yehova . FUNSO : Kodi colinga ca Mulungu kwa anthu ndi dziko lapansi n’ciani ? Inde , tonse , kaya ndise acikulile kapena acicepele , tidzakumana na zinthu zimene zingayese kukhulupilika kwathu kwa Yehova . — Yak . Patapita nthawi , tinakuka ku Estonia n’kukakhala ku Nezlobnaya , kum’mwela kwa dziko la Russia . Kunena zoona , Adamu ndi Hava analibe cifukwa cokhumudwila ndi Mulungu . — Genesis 1 : 28 . ( Ŵelengani Miyambo 10 : 22 . ) OLOŴETSEDWAMO : Yehova ndi Isiraeli wakuthupi ( b ) Kodi cikondi cathu cingayesedwa m’mbali zitatu ziti ? Kodi kukonzekela Cikumbutso kungakhudze bwanji utumiki wathu ? Ricky anafotokoza kuti : “ Tsiku lina usiku pamene ndinali kupita capafupi ndi cipinda ca mwana wanga , ndinaona kuti malaiti anali osazima . Mukacita zimenezi , “ mtendele wa Mulungu . . . udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu ” ndipo mudzatha kukaniza mabodza onse a Satana . — Afil . Popeza kuti Jowana anali mkazi wa woyang’anila cuma ca Herode , anthu amanena kuti iye anali wolemela . Njila zimenezi zingakhale zovutilapo kwa acikulile ena . ( Sal . 128 : 1 ) Pamene muonetsa kuwala kwanu mwa kuthandiza ena kuyamba kutumukila Mulungu , kucita zinthu zolimbikitsa mtendele , na kukhalabe maso mwauzimu , mudzapeza cimwemwe coculuka . ( Machitidwe 3 : 19 ) Zotsatilapo zake n’zakuti , tingaleke kusangalala potumikila Mulungu ndipo tingasiye kulalikila . Nthawi zambili n’nali kulalikila nekha , kupatulako kumapeto kwa wiki . N’nali kuseŵenzetsa makadi aulaliki na galamafoni . Pa kagulu kathu tinali oposa 100 , ndipo pafupifupi hafu anali Akatolika , ena anali a Protesitanti , koma mmodzi cabe anali Mbuda . Mwina mungaŵelenge caputala m’buku la Machitidwe kuti mukhale wacangu mu utumiki . Komabe , tonsefe tingaphunzile za io m’Mau a Mulungu ndi m’nkhani zopezeka m’mabuku athu . Nanga bwanji za anthu mabiliyoni ambili amene anafa asanadziŵe Yehova ndi kum’tumikila ? M’zaka za m’ma 1970 panali kusintha kwakuti mipingo , nthambi , ndiponso likulu lathu ziziyang’anilidwa ndi gulu la abale oyenelela osati ndi munthu mmodzi . Tingaphunzile mfundo zothandiza pa zolakwa za ena , kuphatikizapo za anthu amene anachulidwa m’Baibo . Mau a Cingelezi amene anali kumveka acikale , anawasintha ndi kulembamo mau ena amakono amene amapangitsa Baibuloli kukhala losavuta kuŵelenga ndi kumva , koma sanasinthe tanthauzo lake . PA CIKUTO : Anthu amene amapita kukasangalala ku Tamarindo , malo amene ali m’mbali mwa nyanja ya Pacific m’dziko la Costa Rica , amasangalala akaphunzila kuti mtsogolomu dziko lonse lapansi lidzakhala paladaiso , ndipo mmenemo tizikalima ndi kusangalala Kodi Yesu anaonetsa bwanji kulimba mtima “ atakhala pakati pa aphunzitsi ” m’kacisi ? Nanga Mulungu anaŵalengela ciani ? ” Tiyeni tione umboni wotsimikizila mfundo imeneyi . 7 “ Iye Amapeleka Mphamvu kwa Munthu Wotopa ” Kodi n’ciani cinawacititsa mantha ? Ndipo akulu enawo anavomeleza . 8 : 32 , 33 . Ndipo wakhala akutumikila m’maiko osiyana - siyana pamodzi na mwamuna wake . Ericka anati : “ Tapeza madalitso ambili potumikila mumpingo wa citundu cina , kuphatikizapo mabwenzi . Anthu akubuula , kumva zowawa , ndiponso kufa . Koma kodi gulu locepa limeneli likanakwanitsa bwanji kufikila anthu 60 miliyoni a m’dzikolo , amene anafunikila kuona kuwala kwa coonadi ca m’Baibulo ? Maria anayamba kudwala - dwala , koma mu 1956 anatulutsidwa m’ndende ndipo anauyamba ulendo wopita ku Tulun . 6 : 4 ) Ndipo monga mmene taonela , izi zimaphatikizapo zambili kuposa kuwaphunzitsa cabe zimene Baibo imakamba . Zimaphatikizaponso kuwathandiza kukhulupilila zimene amaphunzila . Ndaphunzila kudalila kwambili Yehova m’mbali zonse za moyo wanga . ” ( Mac . 18 : 26 ; Aroma . 16 : 1 , 2 ) Nkhani zao zocititsa cidwi za zimacititsa m’Malemba Acikristu Acigiriki kukhala okondweletsa poŵelenga . Ndidzayembekezela moleza mtima Mulungu wa cipulumutso canga . 29 - 30 . Izi zinacititsa kuti atumwi ndi abale ena agonjele ku cifunilo ca Mulungu ndi kulandila anthu akunja osadulidwa mumpingo wacikhiristu . ( Mac . Anaonjezela kuti : “ Ndinali kupemphela tsiku lililonse pafupifupi nthawi iliyonse kuti ndikhale wolimba pa cisoni cimene ndinali naco . Komanso sindinafune kupatsa Satana mwai wotonza Yehova mwa kusankha zinthu mopanda nzelu kapena kucita zinthu mosakhulupilika . 4 : 15 , 16 ) Atate wathu wacikondi amafuna kuti tiziona abale ndi alongo athu kukhala ofunika , ngakhale amene aoneka kuti ndi ofooka . Komabe mwa kutiuza dzina lake , Mulungu wacititsa kuti zisakhale zovuta kumuyandikila . Ngati tate akhala kutali ndi banja lake , amalephela kusamalila udindo wake monga mutu wabanja . Limeneli ndi khalidwe limene likuzimililika masiku ano . Masiku anonso , anthu ambili amene anasamukila ku France akuphunzila coonadi . Ngati taona kuti cikhulupililo cathu cayamba kufooka , tiyenela kutengela Petulo . Lembani m’ndandanda wa malemba otonthoza . Zanga zonse zataika ! ” ( 1 Petulo 2 : 21 ) Yesu anakamba kuti munthu ayenela kukonda Yehova ndi mtima wake wonse , moyo wake wonse , ndi maganizo ake onse . Ngakhale kuti aneneli onyenga 400 anatsimikizila Ahabu kuti adzapambana nkhondoyo , mneneli woona wa Yehova , Mikaya , anakambilatu kuti Ahabu adzagonjetsedwa . Ngakhale asanapite ku ukapolo , Aheberi anali kunyalanyazidwa ndi Aiguputo cifukwa ca kusiyana mtundu kapena kusankhana cipembedzo . ( Gen . 11 - 13 . Pambuyo pokambilana naye maulendo angapo , anavomeleza kuti ndinali kukamba zoona . Cifukwa ca kukoma mtima kwake kwakukulu , Yehova amatikhululukila macimo . Koma amacita zimenezo ngati ndife olapa , ndipo tikuyesetsa kulimbana ndi zilakolako zoipa . Panthawiyi anakhala ndi umoyo wosalila zambili n’colinga cakuti asunge ndalama kuti akakhaliletu ku Russia . Namzeze Nthawi ina , Yosefe anali na mwayi wofotokozela mkaidi mnzake zimene zinamucitikila . Ngati ndi conco , sindinu nokha . Munthu wodzicepetsa amadzipenda , kapena kudzisanthula , kuti aone ngati amacita zinthu mogwilizana ndi ciyezo ca Yehova . Zili conco cifukwa timadalila malangizo a Mulungu opindulitsa . 7 : 16 ) Mungacite bwanji zimenezi ? Ma IUD okhala na mahomoni : Pali mitundu yosiyana - siyana ya ma IUD okhala na mahomoni ofanana ni aja amene amapezeka m’mapilisi a cilezi . Ufumu wa Mulungu udzathetsa gwelo la mavuto onse padziko lapansi mwa kusintha mitima ya anthu . Nkhani ya amuna anayi okwela pa mahosi ni imodzi mwa nkhani zodziŵika kwambili m’buku la Chivumbulutso . Anthu ena amati amakhulupilila cisanduliko , koma amaganizanso kuti Mulungu aliko . Sizidziŵika ngati nsombazo zinali kukhala utali wotani akazikonza mwanjila imeneyi . Ndimayamikilanso oyang’anila oyendela osaŵelengeka amene anali kundilimbikitsa . Iwo mwamsanga amayamba kupeleka thandizo la mankhwala kwa munthuyo . Zimenezo zinapangitsa kuti ayambe kulakalaka mkazi wa mwiniyo , ndipo pamapeto pake anacita naye cigololo . ( b ) Kodi Yesu anaphunzitsa bwanji anthu mmene angathetsele vuto la kusankhana mitundu ? Anaona kuti anthuwo am’pandukila . Poyankha , io anagwilitsilanso nchito Baibulo ndi kutifotokozela kuti Yesu si Mulungu ndipo salingana naye . Ndipo Baibo imaonetsa kuti palibe ngakhale mmodzi amene anatsutsa zimene Petulo anakamba , zakuti Davide “ anaonelatu zapatsogolo ndi kunenelatu za kuuka ” kwa Mesiya wolonjezedwa . Davide anacita cigololo ndiponso anapha munthu , koma mneneli Natani anamuuza kuti : “ Yehova wakukhululukila chimo lako . ” — 2 Sam . ( Mat . 24 : 30 ) Nanga abale a Kristu ndi a nkhosa zina adzacita ciani ? PAKATI pa aja amene asamukila ku maiko ena , pali akulu amene atumikila zaka zambili kusamalila nkhosa . ( 1 Sam . 3 : 12 - 14 ) Komabe , ngati makolo amacondelela Yehova na kufuna - funa citsogozo ca Mau ake na mzimu wake , iye amawapatsa nzelu na kuwathandiza kukwanilitsa udindowu . — Ŵelengani Yakobo 1 : 5 . Izi zacitikilapo Akristu ena odzipeleka , cakuti acotsedwa mumpingo cifukwa cakuti sanalape . ( 1 Akor . Mu December 1966 , n’naikidwa kukhala woyang’anila nthambi , ndipo nthawi zambili n’nali kusamalila nkhani zokhudza malamulo . ( 2 Timoteyo 4 : 10 ) Conco , tiyenela kupitiliza kudzifufuza mmene timaonela zinthu za m’dzikoli , ndi kusintha ngati pafunika kutelo . 11 : 5 , 6 , 10 ; 14 : 3 , 4 ) Pamenepa pali phunzilo lalikulu kwa ise . 26 : 51 , 52 . NYIMBO : 46 , 127 Amuna — Muzisangalatsa Akazi Anu 10 Ngati Akristu odzozedwa amenewo anali kuika maganizo ao pa “ mfundo zimene ndi maziko a moyo wa m’dzikoli , ” zikanaonetsa kuti anakana njila ya Yehova yopulumutsila anthu . Patapita nthawi , winanso ananipempha kuti nizichaya baseball m’timu ya dziko lathu la Costa Rica , imene inali ndi anthu osankhidwa kucokela m’matimu wamba . Komabe , io amangolalikila m’chalichi , pa TV , kapena pa Intaneti , mwinanso amangouza ena mmene anaphunzilila za Yesu . Tiyenela kucita ciani ngati taona kuti mapemphelo athu sakuyankhidwa mwamsanga ? Iye anati : “ Ndinakulila m’banja losauka m’mudzi wa ku maphili a Andes . Conco anasintha umoyo wake . Analeka khalidwe losamvela malamulo , kugwilizana ndi anthu aciwawa , ndi kukoka camba . Iyi ndiyo inali nthawi yoyamba kuona dalitso la Yehova cifukwa coika zinthu za Ufumu patsogolo . Izi zingatanthuze kuzilola kutenga ciliconse cimene zifuna . ( Mat . Pamene Yesu anali pa dziko lapansi , anacilitsa odwala , olemala ndi kuukitsa akufa . ( Sal . 32 : 1 , 2 ) Mosakaikila , cilango cinathandiza Davide kukhala m’busa wabwino wa anthu a Mulungu . Mwamuna afotokoza mbili ya moyo wake mkavidiyo kakafupi ka mutu wakuti N’tacoka m’Ndende n’Nakhala na Umoyo Wabwino pa www.jw.org . Buku lakuti The World Book Encyclopedia linakamba kuti Baibulo ndi buku limene “ limakamba za anthu apamwamba ndi otsika , ” komanso “ zolinga zao , zolakwa zao , ndi zipambano zao . ” Wamasalimo analemba kuti : “ Kuyandikila kwa Mulungu ndi cinthu cabwino . ” Paciyambi pa maphunzilo anu , muzikambilana zocitika za m’Baibulo zimene zingathandize wophunzila kuona ubwino wokhala wodzipeleka , wodalilika ndiponso wodzicepetsa . Ife ena tinathaŵila kumadela osiyana - siyana . ” Ndipo tiyeni tizimupempha Yehova kuti atithandize kupitilizabe kucita mbali yathu polimbitsa mgwilizano wa anthu ake . M’Cilamulo ca Mose , muli “ zinthu zofunika kuzidziŵa ndi coonadi ” cokhudza Yehova na mfundo zake zolungama . 1 , 2 . ( a ) Ndi mafanizo ati amene Yesu anauza anzake apamtima ? M’dziko latsopano , Yehova adzagwilitsila nchito mphamvu zake kupeleka zakudya zambili zabwino kwa “ anthu a mitundu yonse ” padziko lapansi . — Ŵelengani Yesaya 25 : 6 . M’malo modziimba mlandu kapena kunamizila ena , bwanji osangocita zilizonse zotheka na kukonza zinthu ? Komabe , atumwi ake anacita mantha ndipo anayamba kukayikakayika m’mitima yao . Conco , pangano la mu Edeni silimangokamba za amene anasonkhezela kupanduka mu Edeni ndi mmene zotsatilapo za kupanduka zidzathetsedwela . Koma limafotokozanso njila yothetsela kupanduka kumeneko . 12 : 1 - 3 ) Imeneyi ndiyo nkhani yoyamba kulembedwa yonena za pangano la Abulahamu , pangano limene Yehova Mulungu anapanga ndi Abulahamu . Mosakaikila ndi Satana . Baibulo limamucha kuti “ mkango wobangula ” amene ‘ afunitsitsa kuti ameze ’ anthu a Mulungu . ( 1 Pet . Kucita zimenezi kudzathandiza kuti mpingo ukhalebe woyela . Cilakolako coipa cikayamba kumela mizu mumtima mwathu , tiyenela kuyesetsa kucicotsa ( Onani ndime 6 ) Koma Yesu anawauza kuti : “ Kunena za zinthu izi mukuzionazi , masiku adzafika pamene sipadzakhala mwala wosiyidwa pano pamwamba pa mwala unzake umene sudzagwetsedwa . ” — Maliko 13 : 1 ; Luka 21 : 6 . Ziyenelanso kulemekeza Ambuye Wamkulu Koposa , Yehova . Iwo anayambanso kuzunza a Loladi . Atsogoleli amenewo anayesetsa kufuna - funa Mabaibo a Wycliffe , ndipo akawapeza anali kuwaononga . Nkhaniyi ifotokoza mmene Yehova waonetsela cikondi cake . TSAMBA 13 • NYIMBO : 8 , 109 14 : 14 ) Mafumu acikanani anali kumuona kuti ndi “ mtsogoleli woikidwa ndi Mulungu , ” ndipo anali kum’lemekeza . ( Gen . Yehova amakhala Mfumu mwa kucita zinthu zoonetsa kuti ali ndi ulamulilo kapena kugwilitsila nchito munthu wina kuti amuimile pocita zofuna zake . Izi zidzathandiza ana kupanga zosankha zoyenela panthawi imene inuyo simungathe kucita zimenezi . Atate ndi akulu awo a Alfred Kugwila nchito zimenezi kumabweletsa cimwemwe , komanso kungakuthandizeni kukhala ogwilizana kwambili na abale na alongo anu . 15 : 13 - 17 , 32 - 37 ; 16 : 15 – 17 : 16 . Nthawi yocepa , ndinafika m’mbali mwa nyanja ku Portugal . Timoteyo anapitila limodzi ndi Paulo , mwamuna wokhulupilika ndi wamphamvu paulendo wautali kwambili . Mngelo anauza Paulo kuti “ Uyenela kukaima pamaso pa Kaisara . ” Kodi Akristu akumana ndi mavuto otani polalikila masiku ano ? Timoteyo anali wacipepele , mwina wa zaka za m’ma 20 , ndipo anali kulemekeza ndi kukonda kwambili Paulo . Tuakacisi twacipembedzo tumapangidwa kuti azilambililamo milungu kapena munthu wina amene io amaona kuti ndi “ woyela mtima . ” Mfundo imene inam’thandiza ipezeka pa 2 Timoteyo 2 : 15 imene imati : “ Cita ciliconse cotheka kuti usonyeze kuti ndiwe wovomelezeka pamaso pa Mulungu , wanchito wopanda cifukwa cocitila manyazi . ” N’ciani cimene taphunzila m’nkhani ino ? Timaphunzilanso kukhala acifundo ndi odekha . 5 : 22 . Kucokela pamene tinayamba kuphunzila coonadi , taphunzila mfundo zambili za coonadi m’Mau a Mulungu , Baibo , m’zofalitsa zathu , pamisonkhano yacigawo , yadela , ndi yampingo . Zoonadi , lonjezo limeneli likutsimikizila kuti nanunso mungapilile . M’zaka 100 zoyambilila ndi masiku ano , kodi amene amatsogolela pakati pa anthu a Mulungu akhala . . . Ganizilaninso za a Joseph , amene akazi ao anamwalila mwadzidzidzi atadwala matenda a kansa . Komabe , zimenezi sizitanthauza kuti mavuto amene amabwela cifukwa colakwitsa zinthu ndi kusankha molakwika adzakhalapo kwamuyaya . Ahabu anali ndi nyumba yaikulu kwambili yacifumu ku Samariya . Tiyeni tikambilane zina mwa zimenezi . ( Mat . 24 : 3 , 21 ) Cisautso cimeneci cidzayamba Yehova akadzaononga “ Babulo Wamkulu , ” ufumu wapadziko lonse wacipembedzo conyenga . Mulungu adzagwilitsila nchito maboma a anthu kucita zimenezi . ( Chiv . 9 : 15 , 16 ) Samueli anadziŵa kuti udindo wake wokhala mtsogoleli watha ndi kuti Yehova anamupatsa nchito yodzoza munthu wina wom’lowa mmalo . Kodi iye adzamucilikiza pa kusintha kwakukulu kumene kudzacitika pa umoyo wawo ? Mfumu Solomo anati : “ Khulupilila Yehova ndi mtima wako wonse . ” N’ciani cinacititsa kuti Adamu ndi Hava asamvele Mulungu ? Lomba , tili na zofalitsa zambili m’cinenelo cathu , ndipo nimasangalala ndi mayanjano acikhristu pa misonkhano ya mpingo ndi yacigawo m’cinenelo camanja ca ku America . Pamene Tatyana anali ndi zaka 16 mu 1994 , apainiya apadela 6 ocokela ku Czech Republic , Poland ndi Slovakia anasamukila ku Ukraine kukatumikila mu mpingo wao . Zimenezi zinayesa cikhulupililo ca Aroni ndi banja lake . Kodi mumaonetsa kuti ndinu woyela mwa kupewa kuyanjana ndi aliyense wa m’banja amene ndi wocotsedwa ? — Ŵelengani 1 Akorinto 5 : 11 . M’dziko latsopano , Mulungu adzathetsa bwanji zinthu zoipa ? Ena mumpingo anali kukamba mau oipa okhudza mmene anali kucitila utumiki wake ndi mmene anali kugwilitsila nchito nthawi yake . Amafunikanso kukhala olimba mtima kuti apewe makhalidwe oipa ndi kuti apange cosankha cobatizika . Akuluwo anafotokozelanso banjalo mfundo zimene zikanawathandiza kuti capamodzi apange makonzedwe ocita kulambila kwa pabanja ndi ana awo aŵili . ( Aef . Koma sitiyenela kuona kuti nchito yathu yakuthupi ndiye cinthu cofunika kwambili mu umoyo wathu . Nthawi zambili , zotulukapo zake zimakhala zakuti anthu amaona kuti zimene timacita n’zabwino . Akadzafunsidwa kuti , ‘ Kodi zilonda zimene zili pathupi pakozi watani ? ’ Mwacitsanzo , kwa zaka zambili , abusa a cipembedzo anali kuuza anthu kuti Mabaibulo awo a Cilatini ni amene anali ndi mawu olongosoka a m’Baibulo . Mose nayenso anali kukhulupilila Yehova . Komanso anali kukonda kwambili Mulungu . Paulo analemba kuti Akhiristu ali “ ngati akufa ku ucimo . ” Ndiye cifukwa cake . Kodi Yefita anacita lonjezo limeneli mopupuluma ? 48 : 17 , 18 ) Timayamikila kwambili kuti Mulungu amatipatsa malangizo acikondi ndi odalilika . Cikondi ndi limodzi mwa makhalidwe ambili amene Mkristu wofikapo amaonetsa . Ngati ndiye mmene zilili m’gawo lanu , bwanji osayesako njila zina zolalikilila ? Panthawiyo , n’nali mlembi wa m’bale Milton Henschel , amene anatumikila pamodzi na M’bale Knorr kwa zaka zambili m’mbuyomo . ( Luka 17 : 5 ) Yesu anayankha atumwi ake m’njila yapadela kwambili pa Pentekosite mu 33 C.E . Iwo analandila mzimu woyela ndipo anamvetsa mozama cifunilo ca Mulungu . Mu October 1984 , tonse tinakaonekela m’bwalo la milandu . Nyengo nayo inali yozizila maningi . ( b ) Kodi cikondi cimene Akhristu oona ali naco pa anthu anzawo n’cacikulu motani ? Ha , ni mwayi waukulu cotani nanga kukhala m’gulu la Yehova ! Onse m’banja ayenela kudziŵa kuti angapewe mavuto mwa kukambitsilana ndi kukonzekela pasadakhale . M’malomwake , anali kutumikila Davide ndi kum’teteza kwa adani ake . — 2 Samueli 10 : 10 ; 20 : 6 ; 21 : 15 - 17 . ( Mat . 6 : 5 , 6 ) N’zoonekelatu kuti cofunika kwambili si mmene anthu amaonela mapemphelo athu koma mmene Yehova amawaonela . Yehova ndiye mnzanu wa conco . 3 Anadzipeleka Mofunitsitsa — ku Taiwan Kenneth M’madela ena , eni nyumba amalemekeza alendo mwa kuwapatsa zakudya zabwino kwambili kuposa zimene iwo amadya . Iye anatiphunzitsa kuti tifunika kukhala ndi cikondi copanda dyela ndi oolowa manja . — 1 Yohane 4 : 10 . kwa Nowa ? 19 : 11 ) Kuzindikila kumatithandiza kukhala ololela . Ndipo iyo idzam’limbikitsa kuti ayambe kuphunzila Baibulo . Monga mmene taonela , Paulo anapwetekedwa mtima poona mmene Ayuda anali kutsutsila uthenga wa Ufumu . Abale ambili amene anadzipeleka anafunikila kulimbana ndi zolepheletsa zina . Mose anaona kuti kudziŵa Yehova kunali kofunika kwambili kuposa cuma ciliconse . Mosataya nthawi banjali linapeleka mafomu ofunsila utumiki umenewu . Iye anali atalonjeza kuti anthu ake adzamasulidwa , ndipo zinacitikadi . Muzisangalala na cilengedwe ca Yehova . Ni malangizo ati a m’Malemba amene anthu onse m’banja ayenela kuseŵenzetsa kuti akalandile mphoto ? Paulo analemba kuti : “ Ndatsimikiza mtima kuti imfa , moyo , angelo , maboma , zinthu zimene zilipo , zinthu zimene zikubwela m’tsogolo , mphamvu , msinkhu , kuzama , kapena colengedwa cina cilichonse , sicidzatha kutilekanitsa ndi cikondi ca Mulungu cimene cili mwa Kristu Yesu Ambuye wathu . ” — Aroma 8 : 38 , 39 . Asayansi ena akuona kuti kwa zaka mahandilendi angapo apitawo , anthu akhala akucita zinthu zimene zasintha dziko lapansi kwambili . ( Luka 12 : 42 ) Ndiponso , amatitsimikizila kuti amamva pamene tipemphela kwa iye . Kodi munthu wotuma mnzake samakhala ndi ulamulilo kuposa wotumidwayo ? ” Koma Anna anasangalala kucita zimene akanatha . Alendo pa Kacisi Wamkulu wochedwa Ise , ku Japan , ndiponso fano lochedwa Grotto ku Massabielle Lourdes , ku France Baibulo limati : “ Pamene tinali ocimwa , Kristu anatifela . ” ( Yoh . 13 : 3 - 5 , 12 - 15 ) Pamafunika khama kuti tikhaledi odzicepetsa na kuonetsa ulemu kwa ena mwanjila imeneyi . ZINGAKHALE zopweteka mtima kuona kuti makolo anu amene kale anali olimba ndipo anali kudzicitila okha zinthu sangathenso kudzisamalila . ( Chivumbulutso 7 : 9 , 13 , 14 ) Kodi a khamu lalikulu ndi oculuka motani masiku ano ? ( 1 Mafumu 18 : 24 , 37 ) ( 5 ) Panthawi imene kunali cilala ndipo mvula inali isanagweko , Eliya anauza Ahabu motsimikiza kuti : “ Pitani mukadye ndi kumwa , cifukwa kukumveka mkokomo wa cimvula . ” Pofika mu 1982 , iye ndi Penny anayamba upainiya , ndipo anatumikila monga woyang’anila dela ku United States kwa zaka 11 kuyambila mu 1986 . Cifukwa Yehova sanapatse anthu ufulu wodziikila okha miyezo ya cabwino na coipa . — Ŵelengani Miyambo 20 : 24 ; Yeremiya 10 : 23 . Izi tingaziyelekezele na zimene woyendetsa ndeke amacita . Kodi pemphelo lingathandize bwanji munthu amene akulimbana ndi maganizo olakwika ? “ Munthu atakhala ndi moyo zaka zambili , m’zaka zonsezo azisangalala . ” — MLAL . Izi sizinacitike mwamwayi . Mwacitsanzo , anafotokoza mmene tingapewele zilakolako zoipa , zimene tingacite ngati tasemphana maganizo na okhulupilila anzathu , kapena ngati m’banja lathu muli mavuto . Adzakondwela kudziŵa kuti kwa zaka zambili citsanzo cake cathandiza atumiki a Mulungu kukhala okhulupilika . ( Ŵelengani Salimo 123 : 1 - 4 . ) ( Aefeso 4 : 23 ) Alex , amene tamuchula poyamba anakambanso kuti : “ Zimene n’nali kuphunzila m’Baibulo zinali monga madzi oyela amene anali kucotsa litsilo langa . Iye anali kusamalila ophunzila ake na kuganizila zosoŵa zawo . Ŵelengani Salimo 45 : 2 . Ngati tipanga zosankha zabwino , timakhala ndi moyo wokhutilitsa panopa ndi kukhala pakati pa anthu amene “ adzalandila dziko lapansi ” ndi kukhala ndi moyo wosatha . ( 2 Mbiri 16 : 1 - 9 ) Tiphunzilapo ciani pamenepa ? Kucita izi kumatipatsa mwayi wolandila madalitso ambili pali pano komanso moyo wosatha m’dziko latsopano la Mulungu . N’cifukwa ciani kutumikila Yehova ndiye njila yabwino koposa ? Koma Mulungu analonjeza kuti adzabweletsa masinthidwe aakulu amenewo . NYIMBO : 38 , 7 ya August 8 , 2000 , masamba 24 - 26 . Koma akambi a nkhani ocokela ku Beteli akabwela , amayi anali kukonda kudzipeleka kuti awasunge kunyumba kwathu . Tikacita zonse zimene tingathe motsatila Malemba kuti tithetse vutolo , tifunika kusiya nkhaniyo m’manja mwa Yehova pokhulupilila kuti iye adzathetsa vutolo pa nthawi yake ndiponso m’njila yoyenela . N’ciani cidzacitika pamene Yesu adzabwela “ ndi mphamvu ndi ulemelelo waukulu ” ? Nzelu zake n’zozama , ndiponso iye ndi wodziŵa zinthu kwambili . Motelo , nthawi imene timakhala ndi Akristu anzathu mu ulaliki , imatipatsa mwai ‘ wolimbikitsana . ’ — Aroma 1 : 12 . Kukamba zoona , mufunika kucita zambili kuposa kungophunzila Baibulo ndi ana anu mlungu uliwonse . Pamene masiku otsiliza awa ovuta ali pafupi kutha , tili ndi cidalilo cakuti Yehova adzapitilizabe kutipatsa ‘ cakudya ca kuuzimu pa nthawi yoyenela . ’ N’cifukwa ciani sitiyenela kuopa masautso a mwadzidzidzi ? ( b ) Kodi zitsanzo za atumiki okhulupilika akale zingatilimbikitse bwanji ? Rakele , mkazi wa Yakobo , nayenso anali kuyembekezela mwacidwi kuona mmene Yehova adzakwanilitsila lonjezo lake kwa mwamuna wake . N’cifukwa ciani kudzicepetsa n’kofunika kuti ticite mwanzelu pankhani ya mavalidwe ndi kudzikonza ? ( Genesis 18 : 1 - 8 ) “ Amuna ” amenewo anali angelo a Yehova . ( Miyambo 17 : 22 ) Ngakhale asayansi amakamba zimenezi . Angawapatse mphamvu ndi nzelu . ( Luka 15 : 11 - 24 ) Zimene Yesu anakamba zokhudza tate wacikondi wa mwanayo , amene anakondwela ataona kuti mwana wake walapa , zimatiphunzitsa mmene Yehova amaonela munthu wolapa . Tikamasinkhasinkha za tanthauzo la fanizo la Yesu limeneli , timazindikila kuti sitiyenela kudela nkhawa kwambili kuti uthenga wa Ufumu udzafikila bwanji mamiliyoni a anthu amene sanalandilebe uthengawo . ( Salimo 83 : 18 ) Komanso amalengeza kuti Ufumu wa Mulungu ndiwo ciyembekezo cokha ca anthu . Ai ndithu . ( 1 Timoteyo 4 : 1 ) Izi zinacitikadi . Yehova anam’patsanso cakudya ndi madzi paulendo wake wa masiku 40 wopita kumwela ku Phili la Horebe . 148 : 12 , 13 . Anafunika kukhala na luso la kuzindikila , kapena kuti luso loganizila nkhani mwakuya kuti aone cimene cinapangitsa vutolo . 6 : 1 , 2 ) Ndipo iye anakamba motsimikiza kuti anali kukhulupilila kuti akufa adzauka . Komabe , makolo ena apeza njila yophunzitsila ana m’cinenelo cawo uku asonkhana mumpingo kapena kagulu ka cinenelo cina . Iwo aphunzila kucotsa “ mtanda wa denga ” m’maso mwao asanacotse “ kacitsotso ” m’maso mwa m’bale wao . Koma kodi zimenezo n’zoona ? Komabe , Baibulo limene lili ndi uthenga wa Mulungu kwa anthu , limatitsimikizila kuti sali patali nafe ndipo amaŵelengela munthu aliyense payekha . Panthawi imodzi - modziyo , mpainiya wina anandipempha kuti ndipite kukalalikila naye ku tauni ina yaing’ono . N’cifukwa ciani timamvela akulu ? M’nkhani yapita , tinakambilana zimene tiphunzilapo pa zimene munthu wothaŵa anali kucita . Tinayamba kukhala pafupi na mzinda wa Grand Junction . Kumeneko makolo anga anali kucita upainiya komanso anali kuseŵenza kwa maola ocepa pa famu . ( Luka 17 : 21 ) Iwo saphunzitsa anthu zakuti Ufumu umenewo ndi boma lakumwamba lolamulidwa ndi Yesu . Koma inu pamwekha muli na udindo wokonza cipulumutso canu , olo kuti mukali kukhala na makolo anu . N’zoonekelatu kuti zaka ziŵili zimenezo zinali zovuta kwambili kwa Yosefe kupilila . Kodi munaganizilapo za zinthu zimene timacita mwacibadwa ? Zinthu monga kupuma , kuyenda , kapena kuchova njinga , timazicita popanda kuziganizila . Koma m’kupita kwa nthawi , Panayiota anakhumudwa kwambili . ( Maliko 13 : 32 , 33 ) Koma timadziŵa zambili zokhudza Paladaiso wamtsogolo kuposa zimene Mose anali kudziŵa . Ndipo ngati mufuna , mungapemphe a Mboni za Yehova kuti akubweletseleni Baibo kunyumba kwanu . Inde , sitiyenela kukayikila kuti Yehova adzatithandiza kukhalabe oyela . Mwina panthawiyo ndi pamene adzazindikila kuti sanakonzekele kubwela kwa Yesu . Zili ngati kuti Paulo anali kuwauza kuti : “ Anthu inu mwapita kale patsogolo , nanga n’cifukwa ciani mukubwelelanso ku zinthu zacabecabe zimene munasiya m’mbuyo ? ” Komanso nthawi zambili amasankha yekha kucita zinthu zoyenela . Iye angakhale akalibe kufikapo poti n’kukwanilitsa maudindo a umoyo wa banja . 13 : 23 . Mungadziŵe bwanji zimene Mboni za Yehova zimakhulupilila ? Nanga ndalama zomangila malo ao olambililapo ndi zothandizila nchito yao yolalikila zimacokela kuti ? Zingatheke ngati muli ndi maganizo oyenela , wokonzeka ndi wofunitsitsa kusintha . Palibe wokhulupilila iye , ndi Mwana wake amene adzakhumudwe . — Aheberi 11 : 6 ; Aroma 10 : 11 . Mwacitsanzo , mungacite bwanji ngati mkulu wakamba mau oonetsa tsankho ? Tisanapeleke umboni wakuti Mulungu aliko , tingacite bwino kumuonetsa kuti nafenso takhudzidwa ndi kumufotokozela kuti sikulakwa kuganiza cifukwa cake timavutika . ( Hab . ( Luka 4 : 43 ) Anafunika kukhala na mphamvu zapadela kuti akwanitse kuyenda na mendo m’madela onse a ku Palesitina kukalalikila uthenga umenewu . Ndipo kuyambila nthawiyo , iye sanaphonyekodi msonkhano uliwonse . Simuyenela kukayikila zimenezi cifukwa m’Baibo muli ulosi wokhudza kuuka kwa munthu winawake , umene unakwanilitsika patapita zaka zambili , ndipo inu mumaukhulupilila . N’naŵelengako kambili - mbili m’zofalitsa zathu za ubale umenewu . Mungam’pemphe kuti aziŵelenga zakumapeto m’buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , kuphatikizapo malemba osagwila mawu . N’zinthu ziti zimene zionetsa kuti mavuto a anthu akuculukila - culukila ? Ndakonza zimenezi ndipo ndidzazicitadi . ” — YES . Onani ndemanga zocokela pansi pamtima za atsikana aŵili amene amakondwela ndi kulambila kwa pabanja . Kupyolela mwa Mwana wake , Yehova watipatsa nchito yolalikila , imenenso mtumwi Paulo ndi ena anali nayo . Ganizilani mmene Adamu ndi Hava anakhalila odzikonda . Louis anati : “ Mu October 2014 , tinakaloŵa Sukulu Yophunzitsa Baibo ya Akhristu Ali Pabanja * ku France . Mwa kuika nchito yocitila umboni patsogolo , timayamikila dzina lathu lopatsidwa ndi Mulungu mogwilizana ndi Yesaya 43 : 10 limene limati : “ ‘ Inu ndinu mboni zanga , ” akutelo Yehova . “ Ndinu mtumiki wanga amene ndakusankhani . ’ ” 7 , 8 . ( a ) Kodi mungatengele bwanji citsanzo ca Yehova ngati munthu wina wakulakwilani ? ( 1 Akor . 7 : 12 - 16 ) Ngakhale kuti mwamuna wosakhulupilila sangatsogolele banja lake pa zinthu zauzimu , iye afunikabe kulemekezedwa cifukwa ni mutu wa banja . Amuna onsewo anali na maina acigiriki . Liu lakuti “ abale ” lingaphatikizepo akazi mumpingo . Malinga ndi Levitiko 8 : 22 - 24 , kodi Yesu anapeleka citsanzo cotani ? N’zoona kuti anthu ena anali kumulemekeza . Kodi ndise otsimikiza za ciani ? Nanga zimenezi zimalimbitsa bwanji cikhulupililo cathu ? N’cifukwa ciani anthu amene amalephela kudziletsa pa zinthu zina sayenela kutaya mtima ? Conco tifunika kudziletsa kwambili kuti tisamapse mtima ndi makhalidwe a anthu oipa . Masiku ano , Yehova akuseŵenzetsa kagulu ka odzozedwa pophunzitsa anthu ake ndi kucenjeza anthu ena cisautso cacikulu cisanafike . Tsiku lina m’madzulo nili ku sukulu , tinakhala pansi ndi anzanga kukambilana za tsogolo . Misozi ikulengeza m’maso mwake , anatikumbatila . Tikambilana ciani tsopano ? ( 2 ) Kodi odzozedwa ayenela kudziona bwanji ? “ Odala ndi anthu amene akumva cisoni , cifukwa adzasangalatsidwa . ” — Mateyu 5 : 4 . Gulu la Yehova lidzapitilizabe kutikumbutsa kuti tizitumikila Mulungu modzipeleka kwambili . Iwo anamva zimene zinacitikazo kwa abale amene anatsala m’basi ija . “ Mwa cikhulupililo , Mose atakula anakana kuchedwa mwana wa mwana wamkazi wa Farao . ” — AHEB . Muziganizila na kutsatila malangizo opezeka m’Mau ake . Mukatelo , ndiye kuti ‘ mukukumbukila Mlengi wanu Wamkulu masiku a unyamata wanu . ’ — Mlal . Koposa zonse , anthu amakwanitsa kupalana ubwenzi na Mlengi . Ena amaona kuti akakhalako ndi udindo winawake ndiye kuti akupita patsogolo . Kale , iye anali kukhumudwa ndi zocita za abale ndi alongo . Ndiyeno , anaganiza zakuti aphunzile za umoyo wa Davide . Kulikonse kumene mukuyang’ana , kuli mdima . Tachulapo kale za ma sitima , magalimoto , ndi ndege . Koma takhala tikugwilitsilanso nchito njinga , mataipilaita , makina olembela zilembo za anthu akhungu , ma telegalafu , matelefoni , makamela , makina ojambulila mau , makina ojambulila mavidiyo , mawailesi , ma T.V . , mafilimu , makompyuta , ndiponso Intaneti . Mama ine mphete zanga ! 14 : 19 - 22 ) Nakonso ku Efeso , Paulo anakumana ndi gulu la anthu okwiya . Petulo anali kukonda nchito yausodzi . Ilo ndi buku lakale koma lili ndi mfundo zamakono . Iye anaonjezelanso kuti : “ Kudziŵa dzina la Mulungu kwandithandiza kukhala naye paubwenzi . ” Ndiyeno anamenya thanthwelo , osati kamodzi cabe koma kaŵili . — Num . Cifukwa cakuti amatikonda , ndipo afuna kutiphunzitsa kuti zinthu zizitiyendela bwino . ( Mateyu 7 : 12 ) Cocititsa cidwi kwambili n’cakuti malamulo a Ufumu wa Mulungu amaongolela maganizo ndi zocita za anthu . Ndiyeno , anagonja ku cilakolako ca uchimo ndi kucita cinthu cimene anali kudziŵa kuti n’coipa . ( 2 Akor . 3 : 1 , 2 ) Tikanakhala kuti sitinaphunzile coonadi , tikanangotsala ndi zithunzi zathu zakale ndi mapepala a mapulogalamu oonetsa kumene tinali kuvinila . Kuti tipeze yankho , coyamba tiyenela kukumbukila kuti Yesu anali kugwilitsila nchito mafanizo pophunzitsa . ( Chiv . 21 : 18 - 21 ) N’cifukwa cake wamasalimo anafotokoza kuti mkwatibwi ameneyu ali pa “ ulemelelo waukulu . ” Cecilie , amene tamuchula poyamba , anati : “ Ndinaŵelenga zinthu zambili pa Intaneti zokhudza Mboni za Yehova komanso ndinamva zinthu zambili zabodza ndi zonyoza anthu amenewa . ( 1 Atesalonika 5 : 17 ; Afilipi 4 : 6 ) Baibulo limatitsimikizila kuti ngati tipemphela kwa Mulungu , “ mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima [ yathu ] ndi maganizo [ athu ] . ” Popeza ndinali wonyada kwambili ndipo sindinali kufuna kuuzidwa zocita , ndinatengeka kwambili ndi maluso anga ndi zinthu zina zimene ndinali kucita . Kodi simunyadila kukhala m’gulu limene limasamalila kwambili anthu ake ? Anali kubisa zolinga zao zoipa . Cimakwilila zinthu zonse , cimakhulupilila zinthu zonse , cimayembekezela zinthu zonse , cimapilila zinthu zonse . ” Tizipemphela kwa Yehova ndi cikhulupililo conse , podziŵa kuti iye amasamala za ife . Iye anafotokoza kuti : “ Nthawi zonse nimafuna kumvetsetsa kuti zinthu zinakhalako bwanji , kuphatikizapo ubongo wa munthu . Koma funso n’lakuti , Kodi tidzakhalako , kodi mudzalandilako mphoto imeneyo ? Kodi ulosi wa Inoki unali wabwanji ? Iwo anali atasintha mothandizidwa na Mau a Mulungu ndi mzimu wake woyela . Mphepo imawombela kumene ikufuna , ndipo munthu amamva mkokomo wake , koma sadziŵa kumene ikucokela ndi kumene ikupita . Kodi kusonyezana cikondi kumalimbitsanso bwanji cikwati ? Conco , makolo citani zimene mungathe kuti muŵete ana anu ndi kuwathandiza kukonda Mulungu . PAMENE titumikila Yehova , timafuna kuti iye atiyanje , si conco ? Tikamaceza ndi abale ndi alongo athu , makamaka aja amene cikhulupililo cao cinayesedwapo , timalimbikitsana mwa cikhulupililo . “ Woyamba anam’patsa ndalama zokwana matalente asanu , waciŵili anam’patsa matalente aŵili , ndipo wacitatu anam’patsa talente imodzi . ” — MAT . Iwo amayamikila thandizo lililonse limene mungapeleke . ( Maliko 11 : 25 ) Kuti tikhale mabwenzi a Yehova , tiyenela kukhululukila ena . — Ŵelengani Luka 11 : 4 ; Aefeso 4 : 32 . Amuna amenewa analemba maganizo a Mulungu osati ao ngakhale kuti anagwilitsila nchito mau awoawo ndi kalembedwe kawokawo ka Ciheberi . N’ciani cinacititsa Mose kupandukila Mulungu ? Pokumbukila utumiki wake pa zaka zonsezo ku maiko acilendo , iye anati : “ Nthawi zonse , Yehova ananipatsa zofunikila panthawi yake . ” Baibo imati : “ Usunge nzelu zopindulitsa ndiponso kuganiza bwino . ( Ŵelengani Salimo 133 : 1 . ) Kuti timvetsetse mfundoyi , tiyelekezele kuti zaka zambili m’mbuyomo , a Mboni za Yehova kapena makolo athu acikhristu anatilalikila uthenga wabwino wa Ufumu . Woyang’anila woyendela wina anapeza njila iyi kukhala yothandiza . Eliezere anakondwela kwambili kuona kuti zinthu zonse zayenda bwino , cakuti tsiku lotsatila m’maŵa , anapempha kuti abwelele ku Kanani ndi Rabeka . ▪ Tumikilani Yehova Popanda Cosokoneza Atumiki otumikila ku maiko ena ndi anchito odzifunila otumikila ku maiko ena amapita kumaiko osiyanasiyana kukathandiza panchito yomanga maofesi a nthambi , maofesi a omasulila mabuku , Nyumba za Misonkhano ndi Nyumba za Ufumu . 12 “ Lilani Ndi Anthu Amene Akulila ” N’ndani wa ise amene ayenela kulimbikitsa mnzake ? Ndi “ paladaiso ” uti amene Paulo anaona pamene “ anakwatulidwila kumwamba kwacitatu ” ? Kucokela paciyambi pa utsogoleli wake , Yoswa anali ndi buku la Mau a Mulungu olembedwa . Mneneliyu ayenela kuti analimbikitsidwa pamene anaona kuti zinthu zayamba kumelanso . Nanji kukamba na mkazi wacisamariya wa mbili yoipa ! Kodi kudzilanga tekha kungatithandize bwanji kukwanilitsa colinga cauzimu ? Cifukwa ca kuba ndi ciwawa , ndinaloŵa m’ndende nthawi zokwanila 18 . 5 : 22 , 23 ) Conco , mzimu wa Mulungu umathandiza panchito yoika abale pa udindo . Yesu anali wopeleka uthenga wamkulu kuposa anthu amene anacitila umboni uthenga wotelo , cakuti anauza otsatila ake kuti : “ Ngati anazunza ine , inunso adzakuzunzani . ” Ricky anati : “ Coyamba tinali kufuna kupeza mpingo umene munali acicepele ocita bwino mwa kuuzimu , kuti mwana wathu Jacob apeze anzake abwino . ” Mwacionekele , kholo linganena kuti lingacite zimene lingathe kuthandiza mwana wake kusiya khalidwe loipa . ( Miy . Palinso zina zimene Satana na ziŵanda zake sangakwanitse kucita . N’kuthekanso kuti iwo anali na vuto la kunyadila mtundu wawo . Anthu ena samvetsetsa lamulo la m’Baibo lakuti : “ Opa Mulungu woona . ” 13 : 22 ; 1 Yoh . 2 : 15 , 16 . N’cifukwa ciani Nowa ndi Akristu oyambilila anapulumuka cionongeko ca m’nthawi yao ? N’nali Woipa Mtima Kwambili ndi Waciwawa 14 Ndani ali m’pangano la Ufumu ? Nanga adzakhala ndi mwai wotani akapitilizabe kukhala okhulupilika ? Iwo satengeka na zokamba za otsatsa malonda kapena zinthu zina zokopa za m’dzikoli . Ndipo amakumbukila mfundo yakuti : “ Wobweleka amakhala kapolo wa wobweleketsayo . ” ( Miy . Tingaonetse bwanji kuti ndise anzelu tikamalalikila kwa anthu othaŵa kwawo ? Kodi n’cifukwa ciani tifunika kupanga zosankha mwanzelu ? KODI MUGANIZA BWANJI ? Mfundo za m’Baibulo zimatithandiza bwanji kuona moyenela udindo wosamalila banja ? ( b ) Mosasamala kanthu za masautso , kodi tiyenela kucitanji ? Ndinali wodzikonda ( C . Pali pano , tikutumikila monga apainiya kumpoto cakumadzulo kwa dziko la England . Patapita nthawi , n’nayamba kudziimba mlandu cifukwa colephela kucita zimene n’naona kuti n’zoyenela . Ni zinthu ziti zimene tingacite zoonetsa kuti timakonda abale athu mumpingo ? ( Yos . 2 : 4 , 5 , 9 , 12 - 16 ) Rahabi anali kukhulupilila kuti Yehova ndiye Mulungu woona , ndipo anali na cidalilo cakuti adzapeleka dzikolo kwa Aisiraeli . Kucokela ali mwana , iye anali kukonda kuŵelenga Baibo . ( Yohane 14 : 8 , 9 ) Kodi kupitila mwa Yesu mungaone ciani za Atate ? Ndaphunzila kukhala munthu wodzicepetsa , womvela ndi wodziletsa makamaka pa khalidwe langa lokhwiya msanga . Zimene limavumbula Dzifunseni kuti : ‘ Kodi ndimakhululukila ena mwamsanga ? Kutsatila mfundo za m’Baibulo za makhalidwe abwino kwathandiza mpingo kukhala woyela . Zimenezi zathandiza anthu kudziŵa kuti Mboni ndi zimene zili ndi coonadi . N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo 3 Kodi cofunika kwambili ni kuyesetsa kukhala wodziŵika kwa ndani ? Iye anakwatiwa ali ndi zaka 19 . Marita anati : “ Mukanakhala kuno mlongo wanga sakanamwalila . ” “ Muzikhala oyela . ” — LEV . Komanso kuposa pamenepo , kumapangitsa kuti Yehova atiyanje na kutidalitsa . — Mac . 20 : 24 , 35 . Mwacitsanzo , iye anakhala umoyo wosalila zambili n’colinga cofuna kugwilitsila nchito nthawi yake ndi mphamvu zake mu utumiki . 37 : 10 , 11 . Koma kodi tiyenela kuyembekezela kuti Yehova adzaticilitsa mozizwitsa monga mmene anacilitsila anthu akale ? Mu 1939 , mlongosi wanga wina wamkulu , dzina lake Marion , anakwatiwa na Bill Danylchuck , ndipo ananitenga pamodzi ndi mlongosi wanga , Frances , kuti tizikhala nawo . ( Yohane 4 : 35 ) Ku Ghana , pa avaleji anthu 120 amabatizika mlungu uliwonse . 1 : 20,21 ) Akatswili a Baibulo ambili amavomeleza kuti dzina lakuti Yesu linacokela ku dzina laciheberi lakuti Yesuwa , limene mbali yake ina inatengedwa ku dzina la Mulungu . Koma amafunitsitsa kugwila otsalila odzozedwa ndi anzao a “ nkhosa zina . ” ( Yoh . 10 : 16 ; Chiv . ( Mat . 6 : 22 , 33 ) Nanga utumiki umenewu wakhudza bwanji wacicepele Aleksey ? N’zoona kuti tili ndi uthenga wabwino umene anthu ayenela kumva . Ali wotomeledwa ndi Yosefe , anapezeka kuti ali ndi pakati mwa mzimu woyela . M’fanizo la matalente , Yesu anaonetsa kuti odzozedwa afunika kucita khama kuti akwanitse maudindo ao acikristu . N’cifukwa ciani anthu ambili zimawavuta kukhulupilila kuti Mulungu wamphamvuyonse angawaŵelengele ? Mafunso aŵa ndi mayankho ake angakuthandizeni kuyelekezela zimene mumaphunzila ku chechi kwanu na zimene Baibulo imaphunzitsa . Kodi mfundo zimenezi tingazigwilitsile nchito bwanji paumoyo wathu ndiponso pothandiza ena ? M’MADELA ena , mipingo yambili imathandizidwa ndi abale ndi alongo ocokela m’maiko ena . Mapemphelo athu angakhale opanda phindu ngati Yehova sanawavomeleze . Wodzozedwayo akaonetsa ‘ zipatso zosonyeza kuti walapa , ’ sangaonetse kuti akunyoza nsembe ya Yesu akadya zizindikilo za pa Cikumbutso . — Luka 3 : 8 . Caka catha , anthu pafupi - fupi 20 miliyoni zungulile dziko lonse anapezeka pa Cikumbutso . Nthawi zonse afunika kumakambilana ndi ana awo . Kumene aliliko , Satana analinganiza magulu a ziŵanda n’kupanga maboma osaoneka , ndipo anapatsa ziŵandazo mphamvu , na kuziika kukhala olamulila dziko . — Aef . Mulungu anati : “ Zipatso za mtengo uliwonse wa m’mundamu uzidya ndithu . ( b ) Kodi kukonda ena kumaonetsa bwanji kuti ndise okhwima mwauzimu ? Posapita nthawi ndinayamba kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza bongo . Nzelu zopezeka m’Mau a Mulungu ‘ coyamba , ndi zoyela . ’ Kodi Danieli anacita ciani ? Ndevu zimenezo zinali kuonetsa ulemu ; sizinali zazitali ndi zosasamalika ayi . ( b ) Ndi liti pamene Akristu anayamba kugwilitsila nchito kwambili codex ? Amakondanso abale ndi alongo , ndipo amadela nkhawa ena . Komabe , nthawi zina zimavuta . Komabe , sin’nafune kuyenda kukakhala ku Nicaragua cifukwa amayi anali kudwala - dwala , ndipo ndine n’nali kuwasamalila panthawiyo . ( Miyambo 22 : 29 ; 31 : 13 ) Koma pamafunika khama kuti munthu akhale ndi luso panchito . Cifukwa cakuti Danieli analimba mtima na kutsatila cikumbumtima cake , Yehova anam’dalitsa mwa kumupulumutsa mozizwitsa kuti asadyewe na nkhalamu . Iwo anafunika kuyembekezela Mulungu kuti ndiye adzathetsa zinthu zopanda cilungamo . ( Yohane 4 : 24 ) Kodi kulambila motsogoleledwa ndi mzimu ndi coonadi kumatanthauza ciani ? TSIKU lina m’maŵa pamene boti inayandikila doko lochedwa Belfast Lough ku Ireland , kagulu ka anthu amene anaimilila pamwamba pa botilo kanaona mapili obiliwila bwino . 1 : 10 ) Mau a Mulungu amatiuza kuika patsogolo Ufumu wa Mulungu mu umoyo wathu . Baibulo limakamba kuti : “ Phunzitsa mwana m’njila yomuyenelela . Ngakhale akadzakalamba sadzapatukamo . ” — Miyambo 22 : 6 . [ Bokosi papeji 12 ] Cilango Cozikidwa pa Baibulo ndi . . . Koma pasanapite nthawi itali , iwo anakumana ndi vuto . Conco , ndapeza cimwemwe cosaneneka . ” Pamene tiyandikila Mulungu ndi kukonda kwambili Mau ake , timayamba kudalila citsogozo cake . Yehova anacenjeza Kaini kuti ngati ‘ sasintha ndi kucita cabwino , ’ adzacimwa . Kukhala ndi mtima woyamikila kumatithandiza kupilila mosasamala kanthu za zothetsa nzelu zimene tingakumane nazo . — Aef . 5 : 20 ; ŵelengani Afilipi 4 : 6 , 7 . Mafumu amenewo ndi Yehosafati , Hezekiya , ndi Yosiya . Acinyamatawa anafotokoza cikhulupililo cao mwaulemu koma mopanda mantha . Kuŵelenga Baibulo mokweza kudzakuthandizani kumvetsetsa ndi kukumbukila kwambili zimene mwaŵelenga Anali kudziŵanso cinenelo ndi cikhalidwe cao . Kodi amamvela bwanji na zimene anasankha ? Yehova amacita umutu wake mokoma mtima ndipo amapewa kudzikonda . Aisiraeli akanakhala munsi mwa Phili la Tabori , zinthu sizikanawayendela bwino cifukwa magaleta ankhondo a Akanani anali kufuna malo afulati kuti amenye bwino nkhondo . Iye anati : “ Ndimayamikila kwambili thandizo limeneli ndipo ndimapeleka ndalama ya mafuta . Kucotsa mimba n’kosagwilizana na zimene Baibo imakamba pa nkhani ya kulemekeza moyo . Zocita zathu ziyenela kuonetsa kuti timalemekeza Nyumba ya Ufumu ndi misonkhano imene imacitika pa malowa . “ Pamalo onse omuzungulila panali powala . Panali cinacake cooneka ngati utawaleza umene umaoneka mumtambo pa tsiku la mvula yamphamvu . ( Chiv . 20 : 12 , 13 ) Anthu amene adzaukitsidwa adzaphunzila mmene angaseŵenzetsele mfundo za m’Baibulo . Ena amakhulupilila kuti Mulungu anaika Satana kukhala woyang’anila ku helo . Anali kutumikila modzipeleka . Miyezo yapamwamba ya Yehova ndi yodalilika . Ngakhale kuti ndife ocimwa , sitiyenela kulola ucimo kutilamulila . Tiyeni tikambilane zimene zinacitikazo . Kukambilana zimenezi kudzatithandiza kudzifufuza pankhani yokhululukila ena , ndi kumvetsetsa mmene kukhululukila ena kumagwilizanilana ndi cilungamo ca Yehova . Timatsegulilatu Baibulo lathu , ndiyeno tikapatsana moni timaŵelenga lemba . ” Pophunzitsa ana , n’cifukwa ciani kuleza mtima n’kofunika ? Ufumu wa Mulungu sudzabwela kudzaocha dziko lapansili , koma kudzacita cifunilo ca Mulungu monga kumwamba cimodzimodzinso pansi pano . 13 : 37 - 43 ) Ndiyeno , Yehova anali kudzaika Yesu kukhala Mfumu yolamulila anthu padziko lapansi . Baibulo limati : “ Mulungu anamuyankha Mose kuti : ‘ Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala . ’ Sukulu ya Gileadi inayamba mu 1943 , ndipo kuyambila nthawi imeneyo , ana a sukulu okwanila 8,500 aphunzitsidwa ndi kutumizidwa m’maiko 170 . Caciŵili , cikondi ca Mulungu ciyenela kutilimbikitsa kukonda abale athu . Ndinali kufunika cilango cotelo . ” — Aheb . Komabe , panacitika zinazake zimene zikanasokoneza ubwenzi wawo . ( Salimo 11 : 5 ) Mlengi amakonda mtendele ndi cilungamo . Koma mogwilizana ndi mau ake aulosi , Mulungu anapulumutsa Aisiraeli kupitila mwa Koresi , mfumu ya Perisiya . Coyenela : Yesetsani kumvetsetsa nkhani yonse , kuphatikizapo kuzindikila zimene mwana wanu angacite ndi zimene sangathe . Tikulimbikitsa abale na alongo ambili odzipeleka kuti ayambe utumiki umenewu kuti aphunzitsidwe na Mulungu . Kodi cifundo cimene Yesu anaonetsa ndi citonthozo cimene anapeleka , zingatilimbikitse bwanji masiku ano ? Wokwelapo akuimila Yesu Khristu . Iye sanakopeseko sinapu kapena kudiloing’iwa penapake . Atumiki onse a Mulungu amene ni anchito a pakhomo a Khiristu , akugwila nchito yocenjeza anthu imeneyi . — Mateyu 24 : 45 - 47 . “ Manja Anu Asakhale Olefuka , ” Sept . Kodi Eliya anaonetsa bwanji kuti anali ndi cikhulupililo colimba mwa Yehova ? Nanga tiyenela kudzifunsa ciani ? Monga takambila kale , cinsinsi cake ni kuphunzila coonadi ponena za Yehova na kulola zimene taphunzilazo kutitsogolela pa zocita zathu zonse . Ngati ndinu mtumiki wacinyamata wa Yehova , kodi cikhulupililo cingakuthandizeni bwanji kusankha zimene mudzacita paumoyo wanu ? Pamene Mboni zimenezi zinali panyumba imene inali itawonongeka kuyembekezela zipangizo zokonzela nyumbayo , zinaona kuti mpanda wa munthu wina wokhala pafupi ndi nyumbayo unali woonongeka . ( 1 Mbiri 29 : 11 , 12 ) Monga Tate woolowa manja , iye amagaŵila cuma cake cauzimu kwa anthu amene amaciona kukhala cofunika . 11 : 2 , 3 ) Mwina Yohane anafuna kudziŵa ngati kudzabwela munthu wina amene adzakwanilitsa zonse zimene Ayuda anali kuyembekezela . Iye wakhala thandizo lalikulu kwa ine . 5 : 19 - 21 . Makolo ayenela kutsatila kwambili mfundo imeneyi . Kodi muganiza kuti vesili likukamba za Ufumu wa Mulungu ? Lembali limati : “ Mulungu anamukweza [ Yesu ] n’kumuika pamalo apamwamba . Ndipo anamukomela mtima n’kumupatsa dzina loposa lina lililonse . ” Pamodzi na apainiya anzanga pa honda yakangolo kumbali Kodi pali cifukwa comveka cokhulupilila kuti Yehova amalamulila zocitika za pa umoyo wathu m’njila ya conco ? Acinyamata ambili amene satumikila Yehova ali ndi umoyo wodzikonda , ndipo amangocita zofuna zao . Anthu onse okuimilani ayenela kukhala ndi fotokope ya DPA lanu . Dziko lapansi lasintha kwambili makamaka kuyambila pa nthawi ya nkhondo yaciŵili ya padziko lonse . Buku ina inati : “ Palibe ciphunzitso coona cacikhristu cimene ni cozikidwa pa Malemba okaikitsa . ” — Our Bible and the Ancient Manuscripts . Komabe , Malemba amatitsimikizila kuti kumwamba na dziko lapansi zidzakhala kwamuyaya . Ndipo kucita zimenezi kungakhale ngati kulimbana ndi mzimu woyela umene umathandiza anthu a Mulungu kukhala mwamtendele ndiponso mogwilizana . — Ŵelengani Aroma 16 : 17 , 18 . Tiyeni titengele Yefita ndi kumvela Yehova . Ngati timatelo , ndiye kuti tikukonzekela kudzakhala ndi moyo wamuyaya m’dziko lolamulidwa ndi Yehova . Izi zinali kunikhumudwitsa kwambili . Koma masiku ano , coonadi cikulalikidwa kwa aliyense . Kodi cikondi ceniceni cimene cimakhala pakati pa mwamuna ndi mkazi n’cotani ? Kodi Mulungu adzacitanji ndi ngozi zosayembekezeleka ? Zinthuzo zalembedwa kale ndipo akudziŵa mmene zidzacitikila . Ayuda anali kuvutikabe pansi pa ulamulilo wa Aroma , ngakhale patapita zaka 33 kucokela pamene Yesu anapeleka cenjezo . ( Ekisodo 23 : 2 ; 1 Atesalonika 2 : 2 ) Ngati mwauzidwa kucita zinthu zimene muona kuti n’zovuta , muzikumbukila citsanzo ca Abulahamu pankhani ya cikhulupililo ndi kulimba mtima . Kudziŵa za mtsogolo kungakuthandizeni kusankha bwino zinthu pa umoyo wanu . 6 : 9 ; 2 Ates . 3 : 13 ) Ngati takumana na zokhumudwitsa kapena ngati timasemphana maganizo kaŵili - kaŵili na munthu wina cifukwa cosiyana zibadwa , kodi timatha kulamulila milomo yathu na kuugwila mtima ? ( Miy . Kodi Stephen amaona kuti anakwanitsa yekha kusintha ? Muziseŵenzetsa zipangizo zamakono . N’zoona kuti abale ndi alongo amene amasamukila kumadela kumene kukufunika alaliki a Ufumu ambili amakumana ndi mavuto . Tingakambe kuti iwo analibe mtima wodzipeleka pocita zinthu zauzimu . Tiyenela kupemphela kwa Yehova kuti atithandize kucotsa maganizo oipa . Kucita zimenezi kumaonetsa kuti timamudalila kwambili . Panthawiyo ndi ocepa cabe amene anadziŵa kuti ciŵelengelo ca Mboni masiku ano , cingaculuke kuposa pa 170,000 . Kudziwonongela . Gianni ndi Maurizio akhala mabwenzi kwa zaka pafupi - fupi 50 . Kukhululuka . . . N’cifukwa ciani tikamba kuti Yehova ndiye mwini zonse ? ( Mlaliki 12 : 9 , 10 ) N’ciani cingatithandize kudziŵa mau abwino ? Tikamapemphela , timamva mmene Baibulo limanenela kuti : “ Yehova ali pafupi ndi onse oitanila pa iye . Panthawiyi , Tera ayenela kuti anali wodwala ndipo sakanakwanitsa kupitiliza ulendowo . Komanso anali wozindikila , kutanthauza kuti anali kudziŵa mmene ophunzila ake anali kumvelela ndi mmene angawathandizile . Nthawi zina , kusankha mwanzelu na kucita zinthu mwacikhiristu kungakhale kovuta . N’ciani cinakhala cotheka cifukwa ca imfa ya Yesu ? Lembali limanena kuti Uziya anacita zinthu zoyenela pamaso pa Yehova kwa kanthawi , koma pambuyo pake “ mtima wake unadzikuza mpaka kufika pom’pweteketsa . ” 35 : 19 ) Mwanjila imeneyi , wakuphayo anali kulipila moyo wake cifukwa ca kupha munthu wosalakwa . Kudzicepetsa kudzakuthandizani kulandila malangizo ocokela kwa makolo anu na Akhristu ena okhwima mwauzimu mumpingo . — Ŵelengani 1 Petulo 5 : 5 , 6 . Kodi Ida amacita ciani polimbana na vuto imeneyi ? Ndipo anthu ambili samakonda kukambitsilana za imfa . Anthu akanapitiliza kudzilamulila , komanso kutsogoleledwa ndi mulungu wopanda cikondi ndi woipa , Satana . Ndipo m’dela limenelo madzi anali kusefukila . Analinso kuyewa acibale ake , ndipo anali kukhala m’cipinda cacing’ono m’hotela . Munthu akandikwiitsa , ndinali kutenga cinthu ciliconse cili pafupi n’kumutema naco . 8 : 16 ; Luka 1 : 19 ; Chiv . 12 : 7 ) Popeza kuti Yehova anapatsa dzina nyenyezi iliyonse ( Sal . 147 : 4 ) , n’zosakayikitsa kuti angelo onse ali na maina , kuphatikizapo mngelo amene anakhala Satana . Kodi mwezi uliwonse mumayesetsa kuphunzitsa anthu Mau a Mulungu ndi kuwalimbikitsa kuti ayambe kum’tumikila ? ( Luka 6 : 13 ; 10 : 1 ) Anali okonzeka kukalalikila uthenga wabwino kwa ena . Iye anali wodzozedwa ndipo anali kudziŵana ndi M’bale Charles T . Russell Ganizilani citsanzo ca José ndi Rose amene anatumikila Yehova mu utumiki wa nthawi zonse kwa zaka zoposa 65 . Kodi makolo naonso angacite motani zimenezi ? Olo kuti ali na zofooka ndipo amalakwitsa zinthu zina monga ife tonse , amayesetsa kukulitsa makhalidwe abwino . Kodi timalalikila uthenga wabwino wa Ufumu mwacangu ? ( 1 Yoh . 2 : 15 - 17 ) Kuti tisakhodwe mumsampha umenewu , tiyenela kusinkhasinkha pa zinthu zabwino zimene tili nazo , ndi kuyamikila Yehova nthawi zonse kaamba ka mwai wokhala anthu ake . — Ŵelengani Salimo 27 : 4 . Kodi mumayesetsa kusunga “ nyumba ” yathu yophiphilitsa imeneyi ili yoyela ? Nditaŵelenga vesili ndinagwetsa misozi poona mmene zinthu zinalili ndi ineyo . A Daka : Inenso ndinaganiza conco . Yehova wapeleka akulu mumpingo wacikristu amene angatithandize kupilila . Satana ndiye amacititsa anthu kugaŵikana ndi kukangana . Pamene niŵelenga mmene Yesu , Paulo , ndi ena anapililila polalikila , kodi nimasinkhasinkha mmene citsanzo cawo cingakhudzile utumiki wanga kwa Yehova ? ’ Mwacitsanzo , mneneli Ezekieli anaona masomphenya oonetsa gulu la Mulungu lakumwamba monga galeta . ( Ezek . 5 : 5 , 6 . Kodi moyo wanga ndidzaugwilitsila nchito motani ? ( Ŵelengani Aefeso 4 : 32 ; Akolose 3 : 13 , 14 . ) “ Uzikonda Yehova Mulungu Wako , ” 6 / 15 ( Aroma 7 : 25 ) Conco , n’zoonekelatu kuti cikondi cimene cinacititsa Yehova kulenga anthu sicinathe , mosasamala kanthu za kupanduka kwa Adamu ndi Hava . Tifunika kuona dzanja la Mulungu pa umoyo wathu ( b ) N’ciani cimatithandiza kupewa mzimu wokonda cuma ? Conco , nikulimbikitsa ena kucita cimodzi - modzi kuti alandile madalitso ambili . Popeza kuti tikuyembekezela zinthu zosangalatsa zimenezi , kodi aliyense wa ife ayenela kucita ciani ? Monga mmene Yesu anakambila , kuukila kwao ‘ kunafupikitsidwa . ’ Koma molimba mtima , Nicolas anauza akulu a asilikali kuti , “ Siningamenye nkhondo cifukwa ndine msilikali wa Khristu . ” Tumapepala tumenetu tunakonzedwa kuti tutithandize kugwilitsila nchito Baibulo paulendo woyamba ndi paulendo wobwelelako . Tiphunzilapo kuti ana amafuna kwambili kukhala ndi makolo ao kuposa kukhala ndi ndalama , mphatso kapena kukhala m’dela lotetezeka . Kodi pemphelo lingatithandize bwanji kulimbana ndi zilakolako zoipa ? Mwacitsanzo , mngelo Gabirieli anauza Mariya kuti adzakhala ndi pakati popanda kugona ndi mwamuna aliyense . Cinali cifukwa cakuti Abulahamu anali ndi cikhulupililo . — Gen . 15 : 6 ; ŵelengani Yakobo 2 : 21 - 23 . N’ciani cimene okwatilana ayenela kupewa ? Mwacitsanzo , Baibulo limanena kuti “ aumbombo ” ndi “ abodza ” sadzaloŵa mu Ufumu wa Mulungu . — 1 Akorinto 6 : 9 - 11 ; Chivumbulutso 21 : 8 . Koma popeza kuti mwini munda wa mpesayo anali kufuna anchito ambili , anapitanso ku msika maulendo angapo kukasakila anchito ena . Koma anali kusamala posankha mwabwenzi . Kucita izi kumatithandiza kuyandikila Mulungu , ndipo iyenso amatiyandikila . — Yak . Baibo imakamba za masomphenya ambili ocititsa cidwi , amene amatithandiza kudziŵa amene amakhala kumwamba . 37 : 12 - 15 . Komabe , pa mphatso zonse zimene Mulungu watipatsa pali mphatso imodzi yoposa zonse . 1 Petulo 3 : 20 , 21 ( b ) Tingacite ciani kuti nsanje isakatimanitse mphoto ? A Daka : Ndi kudzela mwa Yesu . 4 : 6 , 7 ) Mofanana ndi Nehemiya , nthawi zina tingapemphele ca mumtima , ndipo pambuyo pake tingazindikile kuti Yehova watiyankha . ( b ) Nanga n’cifukwa ciani kukhala ndi khalidwe labwino n’kofunika kwa Akristu ? 55 : 22 ; 68 : 19 ) M’caka ca 2018 , nthawi zonse tikapita ku Nyumba ya Ufumu kukasonkhana , tizikumbutsidwa mfundo yofunika kwambili imeneyi tikaona lemba la caka ku pulatifomu . ( b ) N’ciani cimene makolo anali kucita kuti akhalebe olimba mwauzimu ? N’zoona kuti cilango cimakhala coŵaŵa . Koma coŵaŵa ngako ni mavuto amene tingakumane nawo cifukwa cokana cilango kapena uphungu . ( Aheb . 1 : 33 ; 2 : 6 , 7 . Akhristu ambili anali acimwemwe ngako pamene anali kucita upainiya ali acicepele . Satana atatuma openda nyenyezi kuti akaone Yesu na makolo ake , Yerusalemu yense anagwedezeka anthu atamva za kubadwa kwa Yesu . ( Mat . Popeza n’nali kukhulupilila kuti kulibe Mulungu , n’nayamba kumupewa munthuyo . Anakambanso kuti anzake anali kumuona monga wopusa cifukwa analibe cisumbali . Koma Kim anacita bwino kusakhala na cisumbali . Umu ni mmene ine , mwamuna wanga , mlongosi wanga na mkazi wake , tinayankhila pamene tinapemphedwa kuti tikacite utumiki winawake . Tinali kutumizanso magazini kwa anthu amene analembetsa magazini m’maiko osiyanasiyana . Yendani mmenemu . ” ’ Pamene Yesu anali padziko lapansi , analangiza ophunzila ake kuti ayenela kukhala odzicepetsa . Iwo amakamba kuti dziko inapangiwa kuti ikhale malo oyembekezela cabe , podziŵila kuti ndani ali woyenelela kuyenda kumwamba kuti akakhale na moyo kwamuyaya na Mulungu . Mtumiki aliyense wa Yehova angakumane ndi zinthu zimene zingafooketse cikhulupililo cake ndi kumupatutsa kwa Yehova . ( 1 Akor . 15 : 33 ; Col . Nkhani yoyamba idzafotokoza cifukwa cake tifunika kuyembekezela Yehova . Pafupifupi zaka 6,000 zapitazo , cifunilo ca Mulungu cinali kucitika bwinobwino padziko lapansi . NYIMBO : 142 , 129 ( Mlaliki 12 : 13 ) Koma Mulungu safuna kuti anthu amene amam’lambila azicita naye mantha . Ndipo olamulila ena amakhala na zolinga zabwino . Ilo n’loyela kale mokwanila kapena kuti n’lopatulika . Kodi zocitika za Aisiraeli akale ndi za Akristu a m’nthawi ya atumwi zionetsa bwanji kuti Yehova ndi wadongosolo ? Kudzipeleka ni lumbilo limene munapanga kwa Yehova kuti mudzamukonda na kuika cifunilo cake patsogolo kuposa cina ciliconse . Iye akucitila atumiki ake okhulupilika mamiliyoni ambili nchito zazikulu ndi zodabwitsa . ( Zek . Panthawiyo n’nakwiya kwambili cakuti n’nafuna kubwezela , koma n’napemphanso Yehova camumtima kuti anithandize kubweza mkwiyo . Yelekezelani kuti mukuwaona anthu a ku Merozi akungomuyang’ana msilikali woopsa Sisera , pamene akuthamanga kudutsa mumzinda wao , ali yekha ndiponso ali wotopa kwambili . Amatikumbutsa kuti Yehova salekelela zoipa . Dziko linapangidwa mwapadela kwambili cakuti silinapangidwe cabe kuti tizingokhalamo koma kuti tizikondwela ndi umoyo . ( Dan . 1 : 3 - 7 ) Daniel anapatsidwa dzina lakuti Belitesazara . Yehova akutilonjeza kuti adzatiyankha ngati “ tingamupemphe mogwilizana ndi cifunilo cake . ” — 1 Yohane 5 : 14 . Pofotokoza cifukwa cimodzi cimene anthu amavutikila , Baibulo limati : “ Nthawi yatsoka ndi zinthu zosayembekezeleka zimagwela onsewo . ” YELEKEZELANI kuti mukuona nkhondo yoopsa ndi yolemetsa imene inacitika pakati pa asilikali a Aisiraeli ndi adani ao . Masiku ano , makolo angaphunzilepo zambili pa citsanzo ca Loisi ndi Yunike . Iye nthawi zonse amasunga lonjezo lake lakuti adzatipatsa zosoŵa zathu . — Mateyu 6 : 33 . Ndikali kukumbukila mmishonale wina amene anakamba nkhani m’cinenelo ca Cihiri Motu . Mwacitsanzo , padziko lonse lapansi acibale ndi mabwenzi a anthu amene anafa pangozi ya galimoto , amapanga tuakacisi pa malo amene panacitikila ngoziyo . Amacita zimenezi kuti azikumbukila okondedwa ao . Patapita nthawi yaitali , ena a m’banja lathu anafika ku kampu ya anthu othaŵa kwawo m’dziko la Malawi , imene inali pamtunda wa makilomita 1,600 . Ikuthamanga kuti ucifumu wa Yehova ukwezedwe ndi kuti dzina lake liyeletsedwe . Khalidwe limeneli linachulidwa m’mau a Yesu pa ulaliki wake wa pa Phili . ( Num . 27 : 18 - 23 ) Yoswa atatsala pang’ono kutsogolela Aisiraeli kuloŵa m’dziko la Kanani , Mulungu anamuuza kuti : “ Ukhale wolimba mtima ndipo ucite zinthu mwamphamvu . Ayenelanso kukhala woyenelela kuphunzitsa , wougwila mtima pokumana ndi zoipa , ndi wolangiza mofatsa anthu otsutsa . ” Mfumu Hezekiya nayenso “ anapitiliza kumamatila Yehova . ” Mosiyanako ndi Yehosafati , Hezekiya anafunika kupewa kutengela citsanzo coipa ca atate wake , amene anali kulambila mafano . Conco , Rute anasankha mwanzelu . Kwa miyezi 6 , n’nauzidwa kuti nikacititse masukulu angapo , koma sin’napite ndi Mary . Kodi Mose anatsogoleledwa bwanji ndi Cilamulo ca Mulungu ? Komabe , musaiŵale kuti ofedwa amafunika citonthozo nthawi zonse , osati cabe pa nthawi ya zocitika zapadela . Daniel anapita patsogolo mwakuuzimu ndipo anapatsidwa maudindo osiyanasiyana . Paulo anapeleka malangizo othandiza kwambili kwa Akhiristu amene anali kukhala ku Aefeso , mzinda umenewu unali wolemela ndipo unali ndi anthu ocokela ku malo osiyanasiyana . 5 : 16 ) Dzifunseni kuti , ‘ Kodi anthu ena amaona kuti ndine wokhulupilika kwa Yehova ? Pogona ndinali kucita kuiika ku pilo . NYIMBO : 141 , 97 Ngakhale Yesu Kristu tikanangomudziŵa kuti ndi munthu amene anabwela padziko lapansi kudzatifela . Nanga mufunika kucitapo ciani pa zimene Mulungu wakucitilani ? Sizikanatheka kuti munthuyo akaloŵe kumwamba cifukwa ‘ sanabadwenso ’ m’madzi ndi mu mzimu . N’cifukwa ciani kuwayawaya kubatizika n’kulakwa ? Yesu pamodzi ndi olamulila anzake okwana 144,000 adzabwela kudzalanditsa anthu a Mulungu pano padziko lapansi . Njila yabwino yotsilizila mavuto aakulu ndi mikangano pakati pathu , nikutsatila uphungu wa Yesu . Mkazi anali kuona kuti mwamuna wake sanali kutsogolela banjalo pa zinthu zauzimu . Popeza Yesu anakamba kuti mapeto adzabwela ‘ pa ola limene sitiliganizila , ino si nthawi yogona mwauzimu , yofuna - funa zinthu zosatheka za m’dziko la Satana , kapena zimene timalakalaka . ( Mat . Pocita zimenezi io anali kutiganiziladi . Tiyeni tsopano tikambilane mmene zocitika zamtsogolo zimenezo zidzakhudzila aliyense wa ife . RABEKA anayamba kuona malo a miyala pamene anali pa ulendo . Anagwila nchitoyi kuciyambi kwa zaka za m’ma 1200 C.E . , pamene anali mphunzitsi wa pa Yunivesite ku Paris , m’dziko la France . Mkazi wanga anasowa conena cifukwa coganizila kukula kwa udindowo , kuculuka kwa nchito , ndiponso maulendo amene tidzayamba kuyenda . Kuwonjezela pa nchito zathu za cikondi , tingalemekeze Mulungu mwa kucita zopeleka zaufulu . YESU KRISTU anapatsa otsatila ake nchito yaikulu . Cifukwa ca ici , Nowa ndi banja lake anapulumuka pa Cigumula . Amene amapanga gululi anali kale odzozedwa monga ana a Mulungu m’caka cimeneco kapena cakaco cisanafike . — Aroma 8 : 14 - 17 . ( b ) N’cifukwa ciani mwina Yesu anali kudela nkhawa za mgwilizano wa ophunzila ake ? N’zoona kuti Sara anali mlongo wake wa mimba ina . Mayankho a mafunso amenewa atithandiza kudziŵa amene akucita nchito yopulumutsa moyo imeneyi , ndiponso atilimbikitsa kuti tipitilize kulalikila . — 1 Timoteyo 4 : 16 . Mukamatumikila Yehova ndi moyo wanu wonse mudzakhala ndi maluso amene adzakuthandizani kutumikila Yehova m’dziko latsopano . Ngati okwatilana amacita khama kulola Mulungu kutsogolela banja lao mwa kucitila pamodzi zinthu za kuuzimu , io amayandikila Mulungu , ndipo amakondana kwambili . ( 2 Sam . 12 : 7 - 14 ) Pamene tiŵelenga nkhaniyi , tingacite bwino kudzifunsa kuti : ‘ Kodi Davide akanapewa bwanji mavuto amene anakumana nawo cifukwa cocita cigololo na Bati - seba ? Zonse zimene Yosefe anakamba zinacitikadi . ( Gen . 40 : 1 - 22 ) — 3 / 1 , masamba 12 - 14 . Atabwela n’naŵauza kuti apatse moŵa anzanga ena aŵili amene anakamba kuti analeka kumwa mwaucidakwa . 19 : 26 Pa Genesis 5 : 22 pamati : “ Inoki anayendabe ndi Mulungu woona . ” Pamene tiyesetsa kukhala ndi makhalidwe abwino timaonetsa kuti takonzekela kudzakhala m’dziko latsopano kwamuyaya . ( Aheb . Nanga Baraki ndi Debora anacita ciani pamene adani ao anali kubwela ? Posakhalitsa , n’nadziŵa bwino zofunika kucita posamalila udindo wanga . ” 8 : 2 , 8 . Naona kuti kukhala wowoloŵa manja , kwanithandiza kukhala wokoma mtima kwambili kwa anthu ena . Iye anali wobadwila mu mtundu waciyuda umene unali wodzipeleka kwa Mulungu . John Ekrann ( b ) Ni pa zocitika ziti pamene tiyenela kukhala odziletsa ? Ngakhale n’conco , ndine wotsimikiza mtima kukhalabe ‘ msilikali wa Khristu . ’ — 2 Tim . Olemba nkhani zakale amene anakhalako pambuyo pa imfa ya Kristu , anali kufufuza zinthu zilizonse kuti adziŵe zimene zimatanthauza . Kodi mumalaka - laka kukatumikila ku gawo limene kuli olengeza Ufumu ocepa , koma mumakayikila ngati mungakwanitse ? Kodi “ mivi ” ya Kristu idzaoneka bwanji kuti ndi yakuthwa ? ( b ) Kodi mkulu wina amakonzekela bwanji Cikumbutso caka ciliconse ? Nanga imwe mungatengele bwanji citsanzo cake ? Komanso , Paulo anaonetsa kuti kuimba nyimbo za Ufumu capamodzi kungakhale kolimbikitsa . Cifukwa ca thandizo la akuluwo na cikondi cawo , tsopano banjalo likuonetsa kuwala mwauzimu . Ophunzila oyambilila a Yesu anamvetsetsa zimene zimacitika munthu akamwalila . Tili ca pakati - kati pa sukuluyo , M’bale Nathan Knorr anatiuza kumene tinagaŵilidwa kuti tikatumikile tikatsiliza sukulu . Muzisakila mipata yolalikila kwa ena , ndipo muzipempha Yehova kuti akuthandizeni kudziŵa zoyenela kukamba pa nthawi yoyenela . Yehova amatonzedwa ndi mdani wake wamkulu , Mdyelekezi . Kodi Yesu anadzozedwa liti monga Mfumu yamtsogolo ? Pamene Yesu anali padziko lapansi , kodi anapanga makonzedwe otani okhudza ulamulilo wake ? Wosimba ni Olive Matthews Ena amapita kukatumikila kumalo osoŵa . Komabe , iwo “ anacoka pamaso pa Khoti Lalikulu la Ayuda , ali osangalala cifukwa cakuti Mulungu anawaona kuti ndi oyenela kucitilidwa cipongwe cifukwa ca dzina la Yesu . ” ( Mac . Kodi napita patsogolo mpaka kufika pokhala Mkhristu wacikulile mwauzimu ? ( Aef . Ndiyeno Yehova Mulungu anapatsa munthuyo lamulo lakuti : ‘ Zipatso za mtengo uliwonse wa m’mundamu uzidya ndithu . Zimenezi zidzatithandiza kukula kuuzimu . Mwana wathu wamkazi Gulsayra , amene pa nthawiyo anali na zaka 12 , anali kukonda kulalikila anthu opita na njila . Kodi mumapatula nthawi yoŵelenga Baibulo tsiku lililonse ? “ Kuopa Yehova kumatanthauza kudana ndi zoipa . ” Yehova anacititsa civomezi moti Afilisiti anacita mantha . Ngati tilephela kukhazikitsa mtendele ndi abale athu , Yehova sadzakondwela ndi kulambila kwathu . Mau ake amatitsimikizila kuti iye adzathetselatu zinthu zonse zopanda cilungamo . Kukhala wodzicepetsa kudzatithandiza kulimbikitsa mtendele ndi mgwilizano mumpingo . Iye anati : “ Kwa nthawi yaitali n’nali kudziona kuti ndine wacabe - cabe . N’tafika zaka zaunyamata , n’naloŵa m’timu inayake ya baseball . Mukamakonzekela utumiki mwa njila imeneyi , mudzakwanitsa kugwilitsila nchito Baibulo mwaluso kuti mulalikile mogwila mtima . — 1 Akorinto 2 : 4 . Mike ndi banja lake ataŵelenga za abale ndi alongo amene akutumikila kumalo osoŵa , anaganiza zoyamba kukhala moyo wosalila zambili . Abale ndi alongo ambili amene apita kukatumikila ku “ malo osoŵa ” ku Taiwan , amagwilako nchito yophunzitsa ena Cingelezi kuti azipeza zofunikila paumoyo . Kodi nkhani imeneyi idzaononga mbili yabwino ya munthu winawake ? Kumbukilani kuti Yesu anacenjeza “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” kuti sayenela kukhala kapolo woipa . Anthufe tifunika kugonjela ulamulilo wolungama wa Yehova . Panthawi youmika imeneyi madzi anali kucoka m’nsombazo ndipo mcele unali kuloŵa . Koma banjali silinalekele pamenepa . Nkhaniyo inagwilizanitsa “ nthawi zokwanila 7 ” zimene mneneli Danieli analosela ndi “ nthawi zoikidwilatu za anthu a mitundu ” zimene Yesu anakamba . Kodi amuna ayenela kuonetsa motani umutu wao ? Koma kodi munthu amene amakana kuti Mlengi wathu wacikondi ndiye ayenela kukhazikitsa miyezo ya cabwino na coipa , angakhaledi na mfundo zodalilika za makhalidwe abwino ? ( Yes . ( Luka 20 : 9 - 17 ) Nayenso mtumwi Petulo anaseŵenzetsa lemba limeneli pamene anali kukamba na ‘ olamulila aciyuda ndi akulu ndiponso alembi amene anasonkhana pamodzi mu Yerusalemu . ’ Ngakhale n’conco , ciliconse mwa zocitika zimenezi cikanayambitsa cidani ndi kusokoneza ubwenzi wawo na Mulungu . Tsikulo m’maŵa anali ataona Abulahamu * akucoka panyumba , ndiyeno m’madzulo maso ake anali kunjila kuyembekezela mwamuna wake . Kuti muzikondwela , zimadalila mmene mumaiŵelengela . Caka ciliconse , anthu masauzande ambili amabatizidwa kukhala Mboni za Yehova . Tinatumikila pamodzi ku dela la Cornwall , mu mzinda wa New York . M’fanizo la Yesu la mfumu imene inakongoletsa anthu ndalama , kodi iye anaonetsa bwanji kuti Yehova amafuna kuti tizikhululukila ena ? zimaonetsa zinthu zacilengedwe zopangidwa mwa luso lapamwamba kwambili . Koma panthawi imodzimodzi anali kumudela nkhawa , ndipo n’zacibadwa makolo kumva conco . Ngati muli ndi nchito yoyeletsa Nyumba ya Ufumu , bwanji osapempha acicepele kuti museŵenze nao ? Pofuna kuwacenjeza , Yesu anatsutsa mwamphamvu atsogoleli acipembedzo a m’nthawiyo amene anali acinyengo . Mau a Ahabu akuonetsa kuti iye anali ndi maganizo opanda nzelu . Mwamuna wake anamulola . ( Ŵelengani 1 Mafumu 19 : 5 - 8 . ) Mikhail ndi Inga anavomeleza kuti kutumikila ku dela limene kukufunika ofalitsa Ufumu ambili kwawathandiza kuyandikila kwambili kwa Yehova , kukonda kwambili anthu ndi kukhala ndi moyo wokhutilitsa . Paulo anakumbutsa Akhristu a ku Filipi kuti : “ Inu mukudziŵa kudalilika kumene [ Timoteyo ] anaonetsa , kuti monga mwana ndi bambo ake , watumikila monga kapolo limodzi ndi ine kupititsa patsogolo uthenga wabwino . ” ( Afil . Kuonjezela pa kuphunzila cinenelo anacitanso cinthu cina cimene cinamuthandiza . Yosiya “ anapita kukakumana ” ndi Mfumu Neko ya Iguputo , ngakhale kuti mfumuyo inamuuza kuti siinali kufuna kumenyana ndi iye . Mwa ici , atumiki a Mulungu odzozedwa anali kukumana mwakabisila m’tumagulu kukakhala kotheka . Palibe buku ina yacipembedzo imene ingalingane ndi Baibulo . Tizipewanso ngozi poseŵenza , ngakhale pamene timanga kapena kukonzanso malo olambilila . N’ciani cimene “ Adamu womalizila ” adzacita kuti athandize akufa ? Ofalitsa ena aona njila iyi kukhala yothandiza . “ Yandikilani Mulungu , ndipo iyenso adzakuyandikilani . ” — YAK . Nthawi ina ngati mnzanu wa m’cikwati wacitanso zinthu kapena wakamba mau amene akukhumudwitsani , mukadzifunse kuti : 18 : 22 . Nanga imfa idzaonongedwa motani ? Ndinafika ku Vietnam mu July , caka ca 1969 . Ndipo masiku ano , pali kusiyana kwakukulu pakati pa anthu olemela na osauka . Katatu konse , pa Oweruza 4 : 14 , 15 pamakamba kuti Yehova ndiye anathandiza Aisiraeli kupambana nkhondoyo . Nchito yanga panyumbapo inali kucapa zovala na kutola nkhuni . Kiichi Iwasaki , amene anathandiza kupanga ma Yehu amenewo , anati : “ Yehu iliyonse inali ndi tenti ndi batili ya galimoto kuti aziyatsila malaiti . ” * Mokoma mtima , Yesu anamuuza kuti : “ Mwanawe , . . . matenda ako aakuluwo atheletu . ” Kodi N’zotheka Kukhala m’Cikondi Ceniceni ? N’zoona kuti kuphunzitsa ena kumafuna nthawi ndi khama . Mkhristu sayenela kuona pemphelo monga mwambo cabe . Pemphelo si ‘ kacithumwa ’ kothandiza munthu kuti zinthu zimuyendele bwino . Sitiyenela kufulumila kusiya utumiki wathu cifukwa nthawi zina zimenezo zingakhale zosafunikila . Aroma anali kulamulila Yudeya , ndipo likulu la Yudeya linali ku Kaisareya . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mbali zina za cilango cimene cimapelekedwa m’banja na mu mpingo . Mothedwa nzelu , iye anayankha kuti : “ Palibe amene akudziŵa . ” Cifukwa ca kupanikizika ndi kukhala wotopa , mabanja ena amavutika kupeza nthawi yofunikila kuti alimbitse cikwati cao . ( a ) Ndi cenjezo lotani limene Yesu anapeleka ponena za kuodzela ? Pa cifukwa cimeneci , ana anu acinyamata akhoza kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova monga mmene Yesu anacitila pamene anali wacinyamata . Kuzoloŵela . Lemba la Miyambo 14 : 30 limati : “ Mtima wodekha ndiwo moyo wa munthu . ” Pambuyo pake , Abulahamu ndi Loti anazindikila kuti alendowo anali angelo . Anafika pokamba kuti : “ Ndikubweza mau anga , ndipo ndikulapa m’fumbi ndi m’phulusa . ” Pa Ezekieli 18 : 4 , m’Cihebeli liu limeneli ili na mphatikila ya ה ( ha ) kumbuyo kwake , imene ipangitsa liu limenelo kukhala liu limodzi lakuti הנפשׁ ( han·ne’phesh ) . Yosefe anati : “ Kumasulila kwake ndi uku : Nsengwa zitatuzo zikuimila masiku atatu . ( Ŵelengani Salimo 43 : 3 . ) Mkazi ameneyu ndiponso “ ana aakazi a mafumu , ” ndi mbali ya kumwamba ya gulu la Mulungu amene ndi angelo . ( 2 Akorinto 1 : 8 - 11 ) Conco , pemphelo locokela pansi pamtima n’lothandiza maningi nkhawa zikatikulila kapena wina akadwala mwakaya - kaya . Conco , ngati tifuna kuti tikapulumuke pamene dzikoli lidzawonongedwa , tifunika kukhalabe maso . Paulo anapatula nthawi yambili yoceza ndi Timoteyo . Mau ena okuluŵika amene anthu amakamba m’Cizungu anacokela m’Baibo ya King James Version . Pamene uthenga wabwino unayamba kufalikila , Akristu ambili anayamba kukamba Cigiriki m’malo mwa Ciheberi . Ŵelengani Afilipi 4 : 6 , 7 . Nanga mungakonde kuti banja lanu lidzakhale ndi zinthu zambili zodzakumbukila mu utumiki wa Yehova ? Koma Yehova anawononga mizindayo kuti athetse zoipazo . Iye anafotokoza kuti sanafune kuti akabe , cifukwa kuba kukananyozetsa Mulungu . Komabe , panthawi ina , Davide anauza Natani za mumtima mwake monga mmene inu mungauzile mnzanu zakukhosi kwanu . Zotulukapo za kupandukila Yehova n’zakuti anafa , ndipo anabwelela ku dothi kumene anatengedwa . — Gen . Ambili timakonda nchito zathu , ndipo tingakonde kupitiliza nazo kwamuyaya . kwa atumiki ena okhulupilika a Yehova ? Zifukwa ziŵili zoyambilila zionetsa kuti kukwanilitsa zolinga zauzimu kumalimbitsa ubwenzi wa munthu na Yehova . Cifukwa cacitatu cionetsa mapindu amene amakhalapo ngati munthu wadziikila zolinga zauzimu akali wamng’ono . Kucita zimenezi ndi kupemphela mocokela pansi pa mtima , kunatithandiza kukhala olimba mwauzimu . Zinthu Zoipa Zaculuka Smita , * mai wa zaka 35 ku Dhaka , Bangladesh , anali ndi khalidwe lokonda anthu ndi kuwasamalila . Patapita nthawi , boma ya dziko lake inayamba kulola a Mboni kumanga Nyumba za Ufumu . 9 : 18 . Kodi mudzapitiliza ‘ kuyenda na Mulungu , ’ olo ena atakunyozani kapena kukutsutsani , kapenanso ngati mwakumana na mavuto a zacuma oyesa cikhulupililo canu mwa Mulungu ? Mwacitsanzo , munthu wina wochuka m’mafilimu atakhala wandale anati : “ Kudzicepetsa si mbali yanga , ndipo nipemphela kuti kusakakhaleko mbali yanga . ” Komabe , kucita zimenezi n’kuphwanya mfundo za Kaseŵenzetsedwe ka mawebusaiti athu , * ndipo kwabweletsa mavuto aakulu . Nayenso Yehova ali ndi ife . Ni cinthu canzelu kupanga ubwenzi na anthu aconco . Mavesi amenewa amakamba za makhalidwe amene Mulungu sakondwela nao . Koma amakambanso kuti : “ Ena mwa inu munali otelo . ” Tsimikizani kuti mukufunsa mafunso amenewa m’mau anuanu , mokoma mtima , ndi mokopa . Koma musacite zimenezo monga wapolisi . Mu mzinda wa Benguela , apainiya apadela atsogoza phunzilo la Baibo m’cinenelo ca manja , mwa kuseŵenzetsa kabulosha ka Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya . Ngati muli m’ndende cifukwa ca cikhulupilio canu , n’zodziŵikilatu kuti mumauzako ena coonadi mukapeza mpata . Kucita zimenezo kumakondweletsa Yehova . ( Miy . ( 1 Yoh . 2 : 15 - 17 ) Pamene muona zinthu za m’dzikoli , musaiwale kuti mtima wanu ungakunyengeni . — Ŵelengani Miyambo 14 : 15 ; Yer . ( Aroma 12 : 19 ) Ngati tinganyalanyaze malamulo ndi mfundo za Mulungu , zimenezo zingakondweletse Mdyelekezi , ndi kunyozetsa dzina la Yehova . MLONGO wacicepele ku Britain anauzidwa na mnzake kusukulu kuti : “ Zoona munthu wanzelu monga iwe umakhulupilila Mulungu ! ” Tingathandize ena mwa kuwakumbutsa mfundo za m’Baibo kapena kuwapatsa malangizo . Yobu anali kukhulupilila kuti ngakhale atafa , adzakhalanso ndi moyo . Pocita nchito imeneyi , timagwilitsila nchito Baibulo limene ndi mphatso yocokela kwa Yehova . ( 2 Tim . 16 : 21 . Kodi izi zionetsa ciani ? ( Sal . 45 : 4 ) Iye adzapambana pa nkhondo yake mwa kuponya Satana ndi ziŵanda zake kuphompho . Koma pali kacisi wauzimu amene amalemekeza Yehova kuposa nyumba iliyonse . Kuonjezela pamenepo , Yehova anathandiza Yobu kudziŵa mphamvu Zake mwa kumuuza zinthu zina zodabwitsa zimene analenga . 9 : 15 ) Mau amenewa anakambidwa ndi Ambuye Yesu . Apa anali kukamba za mwamuna wina amene anasintha n’kukhala Mkhiristu . Muziŵelenga Baibulo tsiku lililonse ndi kupatula nthawi yocita phunzilo laumwini ndi Kulambila kwa Pabanja . — Ŵelengani Salimo 119 : 32 . Pitilizani kuyandikila kwa iye . Kulimbikitsidwa : Ngati talimbikitsidwa kucita zinthu zinazake , timazicita mwa kufuna kwathu cifukwa tikuona kuti n’zoyenela . Mudzadalitsidwa kwambili palipano ndiponso mudzalandila moyo wosatha m’Paladaiso mmene simudzakhala imfa , “ kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . ” Ciyembekezo cimeneci n’codalilika cifukwa Mlengi wathu ndiye anatilonjeza . Ndipo , ndimawauza za cibwenzi ciliconse m’malo mowabisa . ” N’zotheka kukhala acimwemwe pa nchito yopanga ophunzila , ngakhale kuti ni anthu ocepa cabe amene amamvetsela uthenga wabwino m’gawo lanu . Colinga cinali cakuti munthu wothaŵa azifika mwamsanga ndi mosavuta mumzinda wothaŵilako . ( Num . ( b ) Tidzakambilana mafunso ati ? Kalata imene analembela amai ake usiku umene anaphedwa , inaonetsa kuti anali ndi cikhulupililo colimba kwambili ndiponso kuti anali kudalila kwambili Yehova . Ine ndimafuna kutengela citsanzo cake ndikadzakumana ndi ciyeso cotelo . ” — Onani mau akumapeto . Conco , zoona n’zakuti “ mwa Adamu onse akufa . ” ( Yak . 5 : 11 ) Conco , sitiyenela kukayikila kuti iye adzatidalitsa ifeyo ndi ena onse amene amacilikiza ulamulilo wake . Kupemphela pamodzi na Mkhristu wofedwa ndiponso kumupemphelela n’zofunika kwambili . 3 : 14 , 15 ) Komabe , n’zoonekelatu kuti Abele anali kuganizila kwambili za lonjezolo ndipo anadziŵa kuti winawake ‘ adzavulazidwa cidendene ’ n’colinga cakuti anthu adzakhalenso angwilo ngati mmene Adamu ndi Hava analili asanacimwe . Zimenezi zidzakuthandizani kukhalabe wokhulupilika . — Yohane 14 : 26 . N’zolinga ziti zimene acicepele angadziikile ? Kuti tiyankhe funso limeneli , tiyeni tikambilane citsanzo ca wophunzila wina wakale . Oliver , ni m’bale wocokela ku United States wa zaka pafupi - fupi 40 . Koposa zonse , tidzaphunzila mmene tingalemekezele Yehova Mulungu , Gwelo la ufulu weni - weni . Panthawiyi kukhulupilila Yehova n’kofunika kwambili ngakhale kuti kucita zimenezi kumakhala kovuta . ( Aefeso 5 : 15 , 16 ) Timapitiliza kukhala pa ubwenzi na Mulungu mwa kuona ubwenzi wathu na iye kukhala cinthu cofunika kwambili mu umoyo wathu . — Mateyu 6 : 33 . Koma mofanana ndi Paulo , iwo anakhalabe olimba ndipo sanaleke kulalikila . ( Sal . 26 : 4 ; Miy . 22 : 5 ) Anthu ena amaseŵenzetsa nkhani na zinthu zina zopezeka m’zofalitsa zathu kapena cizindikilo ca jw.org potsatsa malonda . ( Luka 3 : 21 - 23 ; 4 : 14 , 15 , 43 ) Pambuyo pa imfa yake , atumwi ake anapititsa patsogolo nchito yolalikila imeneyi . Kukamba zoona , Yehova watipatsa malangizo ambili kuti zinthu zitiyendele bwino . Tinaucita na mtima wonse ndi mwacimwemwe . ” Ni mapindu ena ati amene timapeza ngati tionetsa cikondi ? Caka catha , tinafalitsa mabuku ndi zinthu zina zofotokoza Baibulo zokwana 4.5 biliyoni . Tinalibenso ciyembekezo coti tikhala ndi moyo . Koma cokondweletsa n’cakuti , Baibulo limatiuza cifukwa cake zinthu zotelezi zimaticitikila ndi mmene tiyenela kucitila tikakumana ndi mavuto . Mpake kuti amafunsa conco . Kumeneko , anamenya mnyamata wina mpaka kumupha cifukwa cakuti anakana kuwapatsa jekete yake . Nthawi zina kupatukana kungakhale komveka . Zimene Koresi anacita zinali zacilendo cifukwa iye sanali kulambila Mulungu wa Ayuda . M’nthawi ya atumwi , Paulo ndi ena anali ndi mphamvu yocilitsa odwala , koma si Akristu onse amene anacilitsidwa mozizwitsa . Malangizo a Paulo Akuti Asapitilize Ulendo wa Pamadzi ( Mac . 27 ) , Na . Muganiza n’kuti kumene tingapeze thandizo na citonthozo ? Pemphelo limathandiza Janet kukhazikika maganizo ndi kulimbitsa ubwenzi wake ndi Mulungu . Diane Yehova amaona kuti zinthu zikutiyendela bwino mu utumiki osati cifukwa coona mmene anthu amakhudzidwila ndi zimene timawaphunzitsa , koma amayamikila khama lathu kaya anthuwo alabadile uthenga wathu kapena ai . — Ŵelengani Luka 10 : 17 - 20 ; 1 Akorinto 3 : 8 . ( Mac . 3 : 19 ; 26 : 20 ) Akulu a m’komiti yaciweluzo ayenela kucotsa mumpingo munthu amene sanaonetse kulapa kwenikweni pa nthawi yoweluza mlandu wake . Nthawi ina , iye anapita kukaceza kunyumba kwa Marita ndi Mariya . Tengelani Khalidwe la Yehova la Cifundo , Sept . Pamene mngelo wa Yehova anaonekela kwa Gidiyoni , iye modzicepetsa anati sanali woyenelela udindowo pokhalanso wocokela ku banja lotsika . NYIMBO : 36 , 11 Paulo anakamba kuti aliyense wakudya mkate ndi kumwa za mkapu mosayenelela , “ adzakhala ndi mlandu wokhudza thupi ndi magazi a Ambuye , ” Yesu Kristu . Tisanacite ciliconse , mwacibadwa timadzifunsa kuti , ‘ Kodi ndidzapeza phindu lotani ? ’ N’cifukwa ciani anthu a Mulungu amadedwa ndi mitundu yonse ? Koma kodi n’cifukwa ciani kusemphana maganizo kumeneku kumacitika ? Ndi uthenga wanji womwe uli m’fanizo la anamwali 10 ? 1 : 17 ) Wamasalimo anachula dzina la Wolamulila ameneyu pamene analengeza kuti : “ Yehova ndi Mfumu mpaka kale - kale , ndithu mpaka muyaya . ” — Sal . ( Eks . 3 : 7 - 10 ) Ngakhale pamene muyenela kuteteza cikhulupililo canu pamaso pa akuluakulu a boma , “ musade nkhawa za mmene mukalankhulile kapena zimene mukanene . Mudzapatsidwa nthawi yomweyo zoti mulankhule . ” ( Mat . Koma anthu onse opanda cikhulupililo anaonongedwa , cifukwa cakuti sanamvele Nowa “ mlaliki wa cilungamo . ” — 2 Pet . Ngati makolo a wacinyamata si Mboni , akulu mumpingo ayenela kumuthandiza mwacikondi kumvetsetsa tanthauzo la kudzipeleka ndi kubatizidwa . ( 1 Akor . 1 : 28 , 29 ) Poyamba , tinagula makina akale ochedwa mimeograph ku boma , ndipo tinayamba kusindikiza zofalitsa zoseŵenzetsa pamisonkhano . ( Luka 4 : 43 ) Iye anaphunzitsanso otsatila ake kuti azipemphela kuti Ufumuwo ubwele . Atumiki a Yehova anatha kucita zonsezi cifukwa cakuti anali ogwilizana . — Genesis 6 : 14 - 16 , 22 ; Numeri 4 : 4 - 32 ; 1 Mbiri 25 : 1 - 8 . Munthu wanzelu kupambana onse anati : “ Nzelu imatsimikizilika kuti ndi yolungama cifukwa ca nchito zake . ” ( Ŵelengani Maliko 4 : 37 - 39 . ) Ndiye cifukwa cake anakamba kuti tifunika kusunga malamulo ake ‘ monga mmene iye anasungila malamulo a Atate ake ndi kukhalabe m’cikondi cake . ’ Dokota wina ku Scotland , dzina lake Derek Cox anati : “ Munthu wacimwemwe amadzadwala matenda ocepa m’tsogolo kusiyana na anthu amene alibe cimwemwe . ” Domitian mng’ono wake ndiye anakhala mfumu . Mwamsanga anamanga cipilala cacipambano polemekeza Tito . 13 : 35 ) Yakobo , m’bale wake wa Yesu , anakamba kuti cikondi ni “ lamulo lacifumu . ” ( Yak . Iye anali kukhulupilila ndi mtima wonse kuti “ Mkhiristu aliyense ali na ufulu komanso udindo woŵelenga na kuphunzila Baibo payekha . ” Ngati ‘ mwayesetsa kuti mukhale woyang’anila ’ kwa zaka zambili , kodi nthawi zina mumadela nkhawa ? Iye amawakonda kwambili ndipo amawateteza , kuwatsogolela , na kuwadalitsa . Conco , zinthu zikasintha pa umoyo wa mwana wosamalila makolo , banja lingapangenso makonzedwe ena . Ena amakamba kuti Mulungu satidela nkhawa . Ndife odalitsidwa kwambili kukhala ndi magazini , mabulosha , mabuku , mavidiyo , ndi Webusaiti yathu , zimene zimacilikiza kulambila koona . Mkwatibwi akumubweletsa kwa Mfumu Mesiya amene ndi mwamuna wake . Ganizilani citsanzo ca Mfumu Yosiya . 1 , 2 . ( a ) Ndi madalitso otani akuthupi amene tikuyembekezela m’Paladaiso ? M’bale Ionash anati : “ Kuti nipeze sitima , n’nali kuuka 04 : 00hrs kuseni - seni , ndipo n’nali kulalikila mpaka 18 : 00hrs , nthawi imene sitima inali kubwelela kwathu . Koma anafunikabe ‘ kusamala nthawi zonse ’ ndi zimene anali kuphunzitsa kuti ulaliki wake ukhale wogwila mtima . Mitengo ya mkuyu inali kupezekanso m’cigawo ca Sefela , malo amene anali pakati pa mapili ndi nyanja ya Mediterranean . Mwacionekele , cikondi ca Mulungu cingatilimbikitse kukhululukila abale ndi alongo athu ndi kuyembekezela nthawi pamene tonse tidzakhala angwilo kwamuyaya . M’nkhani ino , takambilana zimene kukhala munthu wauzimu kumatanthauza . Kodi tingati Kenneth na Filomena analakwitsa kukhulupilila kuti Mulungu anawathandiza kupitila mwa mngelo , mzimu Wake woyela , kapena mphamvu yake yogwila nchito ? Nthawi zina , nchitoyo imakhala yotopetsa ndi yosasangalatsa kwenikweni . Mwamuna wina wokwatila ku South Africa anati : “ Timayesa kutsatila mfundo ya pa Luka 6 : 31 m’banja lathu . PA April 28 , 2013 , mumzinda wa Nagoya , ku Japan munali msonkhano wapadela . Anthu anasangalala pamene M’bale Anthony Morris wa m’Bungwe Lolamulila analengeza za kutulutsidwa kwa buku lochedwa The Bible — The Gospel According to Matthew ( Baibulo — Uthenga Wabwino wa Mateyu ) m’Cijapanizi . Kulimba mtima ndi khalidwe lofunika ngako kwa Akhristu . Monga alengezi a Ufumu , ndi zolinga za kuuzimu ziti zimene tingakhale nazo ? Tifunika kukhala okonzeka cifukwa afika posacedwapa . Amam’thandiza kuyambila ali wakhanda , kuti azikonda kutsatila mfundo zapamwamba za Yehova za makhalidwe abwino . Titangofika kumeneko , tinafufuza kumene kunali a Mboni za Yehova . * Lipoti ya mu 1949 yocokela ku ofesi ya nthambi ku Mexico inati : “ Ngakhale kuti abale amakumana ndi mavuto , saleka kukonda zinthu zauzimu . Takamba conco cifukwa , pambuyo pa msonkhano uliwonse waukulu , kwa nthawi yaitali abale amakonda kukambilana zimene anaphunzila pa msonkhanowo . Komanso , funso limene abale amakonda kufunsa n’lakuti , N’liti pamene tidzakhala na msonkhano wina waukulu ? ” Kodi acinyamata ndiponso tonsefe tiyenela kuyamikila ciani ? ( 2 Timoteyo 3 : 1 ) Ambili akukumana ndi mavuto a zacuma , kutha kwa mabanja , nkhondo , matenda oopsa amene afala , ndi ngozi zacilengedwe kapena zimene zimacitika cifukwa ca zocita za anthu . Patrick LaFranca Cifukwa cakuti anthu akawatamanda , ndiye kuti akulandililatu mphoto yawo yonse . Mwacitsanzo , Mfumu Davide anasankha Alevi 4,000 kuti aziimba nyimbo zotamanda Mulungu pa zocitika za pa kacisi zokhudza kulambila . Abale na alongo ambili anali otangwanika ndi nchito yomanga likulu latsopano la Mboni za Yehova ku Warwick ku America . Ndiponso tidzalimvetsetsa Baibulo , moti m’Paradaiso tidzayamba kucita zinthu mwacikondi kwambili , ndi mwaulemu kwa anzathu . Iye anadziŵa kuti Yesu wafa Pilato asanadziŵe . M’nkhani izi tikambilana zitsanzo zabwino ndi zoipa ndiponso mfundo zimene zingathandize acinyamata ndi acikulile omwe kusankha zocita mwanzelu . Muziona makhalidwe abwino mwa ana anu acinyamata ndipo muziwayamikila Kodi timaona abale ndi alongo athu kuti akali kuumbidwa ndi Mulungu ? Ponena za nthawi imene iye anali mbeta , Bill amene tam’chula poyamba anati : “ Zakazo zinadutsa mofulumila cifukwa ndinagwilitsila nchito nthawiyo kutumikila Yehova monga mpainiya . ” Palinso malangizo a mmene mungacitile daunilodi JW Laibulale Ŵelengani Salimo 45 : 5 . Ndinali ndi njala yofuna kudziŵa mayankho a mafunso amene ndinali nao . Mzimayiyo atamvetsetsa zimene Baibo imakamba pankhaniyi , posapita nthawi anabatizika . Anthu 2,300 anadzaza holo yaikulu ya Osaka Asahi kuti amvetsele nkhani yakuti , “ Ufumu wa Mulungu Wayandikila . ” Padziko pali mavuto ambili . Mu 2006 , pokambilana ndi mabungwe a zipembedzo za Roma Katolika , Papa Benedict wa namba 16 anaonetsa kuti umbeta ni “ mwambo umene unayamba kale kwambili , cifupi - fupi nthawi ya Atumwi . ” 2 : 11 ) Tikadziŵa bwino njila zacinyengo za Satana , sicikhala covuta kukhalabe maso ndi oganiza bwino . 1 : 23 . Koma ngati pali nkhani zina zimene zafala m’gawo lanu , konzani ulaliki wogwila mtima wogwilizana ndi zimene anthu akuganiza . Ngakhale zili conco , io afunika kukhalabe maso mpaka iye atabwela kapena kufika . Buku la m’Baibulo limeneli limafotokozanso za anthu anai okwela pa mahachi . Ngakhale kuti cikhalidwe cao cinali cosiyana ndi cathu , tikhoza kuzindikila kuti aŵiliwa anali kukondana kwambili . Komabe , mu 1971 , zinadziŵika kuti bungwe lolamulila lisiyana ndi Watch Tower Society , imene imayang’anila nkhani zokhudza malamulo . Palibe ngakhale mmodzi wa ife amene akanatha kulipila dipo limene linali kufunikila kuti timasuke ku ucimo ndi imfa . Pambuyo pake , Satana anacititsanso atumiki okhulupilika a Mulungu kukhala ndi maganizo odzikonda . — Yobu 1 : 9 - 11 ; 2 : 4 , 5 . “ Musaope , kagulu ka nkhosa inu , cifukwa Atate wanu wavomeleza kukupatsani ufumu . ” — Luka 12 : 32 . N’nali Kukonda Baseball Kuposa Cina Ciliconse Koma mungafunikile kusamala . Mau amenewa anandikhudza kwambili . Koma n’nali kufuna kumuthandiza cifukwa nimamukonda . ” ( Chivumbulutso 2 : 7 ) Mzimu woyela ungatithandize kulimbana ndi ziyeso ndi kulalikila molimba mtima . Kodi tingapewe bwanji kukodwa mu msampha umenewu ? Citsanzo 3 : Tikakumana ndi munthu amene amakhulupilila kuti anthu onse abwino amapita kumwamba . Cimeneco cinali kudzakhala cizindikilo “ ca mapeto a nthawi ino ” kenako “ mapeto adzafika . ” ( vesi 3 , 14 ) Zizindikilo zimenezi zikuphatikizapo nkhondo zikuluzikulu , njala , zivomezi m’malo osiyanasiyana , kusamvela malamulo , kuzilala kwa cikondi , ndi abusa onama . ( Miyambo 3 : 32 ) Ngati timvela Mulungu , tingakhale mabwenzi ake . Baibulo Limasintha Anthu 14 Paulo anapempha Timoteyo kuti adulidwe , ndipo iye anavomeleza , osati cifukwa cakuti cinali ciyeneletso kwa Akristu , koma cifukwa cakuti Paulo sanafune kuti Ayuda amene anali kuwalalikila azimutsutsa cifukwa coyenda ndi mnyamata amene atate ake anali munthu wakunja . — Machitidwe 16 : 3 . N’kutheka kuti mwina zimenezi zinacititsa Yosefe kukonda kwambili “ Mulungu . . . wa anthu a moyo ” amene ndi wopatsa . ( Yobu 14 : ​ 1 , 2 ) Baibulo limaonetsa kuti ngakhale anthu anzelu kwambili anafunsapo funso limeneli . ​ — Ŵelengani ­ Mlaliki 2 : ​ 11 . Ngati ndimwe Mkhristu wacicepele , bwanji osakhala na colinga codziŵana bwino na acikulile mumpingo mwanu ? Nyanga zimenezi zikuimila maulamulilo onse andale amene amathandiza bungwe la United Nations limene likuimilidwa ndi “ cilombo cofiila kwambili . ” — Ŵelengani Chivumbulutso 17 : 3 , 16 - 18 . Mwina mukanaganiza kuti iwo ali monga dothi lolimba . Monga mmene taonela zitsanzo pamwambapa , anthu ambili samvetsetsa mavesi ena amene amaŵelenga m’Baibo . Kumeneko , Timoteyo analimbikitsa Akristu okhulupilika potsatila zimene anaphunzila kucokela kwa amishonale anzake . — 1 Atesalonika 3 : 1 - 3 . Koma Baibulo limakamba kuti : “ Inunso amuna , pitilizani kukhala ndi akazi anu mowadziŵa bwino . ” Mosiyana kwambili na ufulu uliwonse wocokela kwa anthu , mzimu wa Yehova ungatimasule ku ukapolo wa ucimo na imfa , ndi ku ukapolo wa cipembedzo conama na miyambo yake . Thandizani mwana wanu wacinyamata kupeza mabwenzi abwino mumpingo ( Onani ndime 14 ) Mmene Masomphenya a Zekariya Amakukhudzilani , Oct . Nkhani zimene zimapezeka mu Nsanja ya Olonda za mutu wakuti “ Baibulo Limasintha Anthu ” zili ndi zitsanzo zambili zocititsa cidwi za anthu otelo . Yelekezelani zinthu zimene anthu anali kuona kuti ndi zoipa kwambili m’ma 1940 ndi 1950 , ndi zimene zikucitika masiku ano m’malo anchito , pa nkhani ya zosangulutsa , zamasewela ndiponso kavalidwe . Nkhani yotsatila idzafotokoza mmene nchitoyi ikucitikila masiku ano . Mofanana ndi Akristu a m’nthawi ya atumwi , Akristu ambili masiku ano amaika ndalama pambali kuti akaponye m’bokosi la zopeleka zaufulu ku mpingo wao pocilikiza nchito yapadziko lonse . Komabe , panali kufunikila makonzedwe oyenelela kuti io akalamulile ndi Yesu mu Ufumu wake monga mafumu ndi ansembe . N’ciani cingatithandize kutsanzila nzelu za Mulungu ? Timafunika kuyamba ndife kuyandikila Mulungu ngati tifuna kuti iyenso atiyandikile . Nthawi zambili , n’nali kumenyana ndi anthu pogwilitsila nchito mfuti . Kangapo konse , anzanga ananimenya kwambili n’kunisiya panjila poganiza kuti nafa , ndipo magazi anali kuyendelela thupi lonse . 31 : 31 - 33 . Pambuyo poona masomphenya 8 , Zekariya anacita zinthu zokhala na tanthauzo la ulosi , zimene zinalimbikitsa anthu a Mulungu amene anali kumanga kacisi wake . Satana anatsutsa ufulu wa Mulungu wolamulila cilengedwe conse . 28 : 19 , 20 ) Kuphunzitsa mwanjila imeneyi n’kumene Yehova amafuna , cifukwa kumakonzekeletsa ophunzila kuti nawonso akathe kupanga ophunzila a Khristu . Kodi kulalikila kumaonetsa bwanji kuti tili ndi cikhulupililo ? Udalitsike cifukwa ca kundigwila lelo kuti ndisapalamule mlandu wamagazi ndi kudzipulumutsa ndekha ndi dzanja langa . ” — 1 Sam . ( Ŵelengani Aroma 12 : 1 . ) Fotokozani mmene tingaonjezele cikhulupililo cathu . Nimamuyewa ngako ! Coyamba n’cakuti nthawi zina tingafunike kuthaŵa ngati tayesedwa kuti ticite chimo . Taganizilani mtumwi Paulo , iye anakhudzidwa kwambili ndi nsembe ya Yesu moti analemba kuti : “ Ndikukhala mokhulupilila Mwana wa Mulungu , amene anandikonda ndi kudzipeleka yekha cifukwa ca ine . ” 45 : 4 . Ena amatumikila pa Beteli , ena amagwila nchito yomanga kapena yadela . Zotsatilapo zake zinali zakuti m’baleyo anakwanilitsa colinga cake cocita upainiya wa maola 30 . 4 : 6 ) Kuzindikila zosoŵa za eninyumba ndi zimene amakonda , kudzatithandiza kusankha mau athu moyenelela . Iyi inali imodzi mwa nkhani zimene adani a Yesu anakambapo pofuna kupeza cifukwa Yesu na ophunzila ake . Mosiyana ndi mizinda yambili imene Paulo anapitako , mumzinda wa Filipi munalibe sunagoge wa Ayuda ngakhale mmodzi . Yehova analankhula ndi anthuwo “ pa nthawi ya kamphepo kayeziyezi . ” Kuwonjezela pa kuŵelenga Baibo na mabuku athu ozikidwa pa Baibo , n’ciani cina cimene cingatithandize kuti tizikonda kwambili coonadi ? 8 : 1 ) Kodi cimamangilila bwanji ? Mkulu wina wa asilikali a ku Germany anakamba kuti cimodzi cimene cinacititsa dziko lawo kugonja pa nkhondo yoyamba ya padziko lonse n’cakuti , anthu “ anapusitsidwa ndi mauthenga abodza ocokela kwa adani awo ngati mmene njoka imapusitsila kalulu . ” Satana amafalitsa mabodza pofuna kutigaŵanitsa ndi kutigonjetsa . Kodi kufunsila kwa olosela ndiye njila yodalilika yodziŵila zakutsogolo ? Kodi mau amene Paulo anagwilitsila nchito akuti “ maziko olimba a Mulungu ” ndi ofunika motani ? Nanga zimenezi zinam’khudza bwanji Timoteyo ? Kukonda kudela nkhawa kapena kudandaula pa zinthu zimene sitifunika kuda nazo nkhawa , ngakhale pa zinthu zomveka kungavutitse cabe maganizo a munthu ndi kumulepheletsa kuganizila zinthu za kuuzimu zimene ndiye zofunika kwambili . Pokamba za liwu limene linamasulidwa kuti “ kukoma mtima kwakukulu , ” katswili wina anakamba kuti : “ Mau amenewa makamaka amakamba za mphatso yaulele imene yapatsidwa kwa munthu amene sanaiseŵenzele , ndiponso amene si woyenelela kuilandila . ” 103 : 10 ) Koma pali mapindu ena amene timapeza ngati tipewa ‘ kupsa mtima . ’ Popeza kuti ana a Nowa anayamikila colowa cao cakuuzimu , io anali ndi mwai wopititsa patsogolo mtundu wa anthu ndiponso kubwezeletsa kulambila koyela padziko lapansi loyeletsedwa . — Gen . * Zimakhala zopweteka mtima kwambili kwa ana ang’onoang’ono akasiidwa kwa nthawi yaitali . N’ciani capangitsa Akristu ena kucita chimo ? Nkhani ziŵilizi zidzatithandiza kuti tiziyamikila kwambili Baibo . Zidzatithandizanso kuti tizikonda kwambili Mlembi wake . ( 1 Pet . 2 : 21 ) Mofanana ndi Akristu a m’nthawi ya atumwi , nafenso tingakhudzidwe ndi maganizo onama , nzelu zadziko , ndi kukonda cuma m’dongosolo ili la Satana . Mfumu ya nzelu Solomo inatikumbutsa kuti : “ Galu wamoyo ali bwino kuposa mkango wakufa . ” Mauwa angatilimbikitse kwambili kuti tikapulumuke cisautso cacikulu , ndiponso angatithandize kukonzekela kudzakhala m’Paradaiso . Husai anali wolimba mtima ndipo anaika moyo wake pangozi mwa kumvela Davide ndi kukhalabe wokhulupilika kwa Yehova . Conco , masomphenya amenewa akuonetselatu kuti onse amene akulandila ciitano cakuti “ bwela ” ali ndi udindo wolalikila kwa ena . * Maphunzilo amenewa amathandiza anthuwo ‘ kukhala atsopano mu mphamvu yoyendetsa maganizo ao . ’ USIKU wakuti maŵa adzaphedwa , Yesu anakambilana na atumwi ake kwa nthawi yaitali , ndipo anawatsimikizila kuti amawakonda ngako . Yehova watipatsa ‘ zilizonse zabwino ’ kuti atithandize pa nchito yolalikila . Ndithudi , mau akuti “ wovuta kumvetsa ” ndi oyenelela . Simon , wa zaka 22 , anasamukila ku cilumba ca Palau mu 2007 . Atafika kumeneko , anaona kuti ndalama zimene anali kupeza zinali zocepa poyelekezela ndi zimene anali kupeza kwao ku England . M’mau ena , cikondi cilibe malile a macimo amene tingakhululukile ena . Yefita analinso msilikali wolimba mtima , pamene Hana anali mzimayi wodzicepetsa . M’cinenelo ca Cibiribiri 2 , 3 . ( a ) Kodi kuganizila zinthu zimene sitinazione kungatithandize bwanji ? Zipangizo zimenezo zidzakhala zamahala . Kuciyambi kwa kalata yake yaciŵili yopita kwa Akorinto , Paulo anakamba za ulemelelo umene Mose anali nawo atatsika m’phili la Sinai pambuyo poonekela pamaso pa mngelo wa Yehova . Ngakhale kuti munthuyo anali kudziyang’ana mosamalitsa pagalasi , anali ndi vuto . Koma mu 1992 , n’nayesako kulalikila kwa maola 60 kwa mwezi umodzi . Ine n’nali kufuna kuti nizigwila nchito yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu . Ndinali kuganiza kuti , ‘ Ndingayeseko kuletsa anthu nkhanza koma osati nkhondo . ’ N’ciani cingatithandize kukhala na mtima wofunitsitsa kudziŵika kwa Yehova osati ku dziko ? 6 : 11 ) Kapena kuti : “ Mutipatse cakudya cathu calelo malinga ndi cakudya cofunika pa tsikuli . ” Ngati timalemekeza malo athu olambilila , anthu ena amene si Mboni amaona zimenezi . 12 : 1 . Mavuto ena mu umoyo , amakhala mwina kwa zaka zambili . Angayambe pang’ono - pang’ono ife osazindikila . Koma Yehova wanithandiza kutumikila monga mkulu na kuphunzitsa anthu ophunzila kwambili kuti adziŵe coonadi ca mtengo wapatali . ( Onani ndime 3 ) Wosungila mibadwo masauzande kukoma mtima kosatha , wokhululukila zolakwa ndi macimo . ” ( 2 Mbiri 36 : 15 ) Ifenso tifunika kucitila cifundo anthu oona mtima amene angathe kulapa macimo awo kuti Mulungu ayambe kuwakonda . Kucita zimenezi kudzatithandiza kuti tiyambe kumukonda kwambili . Conco tikapezeka pamisonkhano , timamvetsela kwa Yehova ndi kuona cikondi cake , ndipo timamuyandikila kwambili . Koma m’zaka zapakati pa 1947 ndi 1958 , pa cisumbu cimeneci , panali akaidi oposa 100,000 . Pa akaidi amenewa panali zigaŵenga zacikomyunizimu , anthu oganizilidwa kuti ndi zigaŵenga zacikomyunizimu , ndi ena amene poyamba anali asilikali oukila boma . Komanso panali Mboni za Yehova zambili zokhulupilika . Funso loyamba n’lakuti , n’cifukwa ninji Yesu ananena za ciukililo ca kumwamba poyankha Asaduki , amene mwina anali kuganiza za ciukililo ca padziko lapansi ? 91 : 14 . Maurizio sanali kunimasukila mmene anali kucitila poyamba . Ndipo ngati timamvela mau a Yehova , tidzapewa kumvetsela ampatuko . — Miy . Pa avaleji , munthu amene amakoka paketi imodzi ya fodya tsiku lililonse , amaloŵetsa nikotini woculuka kwambili m’thupi lake kuposa mankhwala ena onse osokoneza ubongo . Muzipempha Yehova kuti amudalitse . ( Onani pikica pamwamba . ) ( b ) Kodi mtumwi Paulo akutikumbutsa ciani ? Nanga zimenezi zibweletsa mafunso ati ? “ Musaiŵale Kuceleza Alendo , ” Oct . Nanga anakhalako bwanji ? Kodi amagwila nchito yabwanji ? Munthu wina yemwe sanali Mboni anati : “ Ha ! Koma ici ndi cipembedzo cacilendo . Ndithudi , Yehova amasangalala ndi khalidwe labwino limeneli . — Mat . M’dzikoli , anthu olungama ni ocepa kwambili poyelekezela ndi anthu oipa . Parkin ) , Aug . Kodi acinyamata ena agwilitsila nchito bwanji nthawi yao kutumikila Yehova ? Koma m’zikhalidwe zina , anthu amayamikila ngati alendo akambilatu kuti adzabwela kudzawacezela . Lidzakhaladi phwando losaiŵalika la ukwati . ( Yohane 3 : 16 ; 1 Yohane 4 : 8 ) Komabe , cifukwa ca mavuto amene mwakumana nao pa umoyo wanu , zingakuvuteni kukhulupilila kuti Yehova amakukondani kwambili . Ngati mufuna kudziŵa zambili , tinikani pa mau akuti “ Citani Copeleka ku Nchito Yathu ya Padziko Lonse ” pansi pa peji yoyamba pa jw.org , kapena mungalembe kalata ku ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova ya m’dziko limene mukhala . Kuwonjezela apo , Adamu ndi Hava sakanabeleka mwana wangwilo . Ni mmene zinthu zinalili mu umoyo wa Mirjana . Pamene anali mtsikana , anali na luso ngako pa zamaseŵela . N’zoonekelatu kuti iye anali kukonda kuuza ena coonadi cimene anaphunzila kwa Bwenzi lake lapamtima , Yehova . ( Mat . 10 : 32 , 33 ) Yosefe sanam’kane Yesu , koma anali kuopa kuvomeleza pamaso pa anthu kuti anali kum’khulupilila . Pa October 27 , 1973 , tinakwatilana ndipo M’bale Knorr ndi amene anatikambila nkhani ya cikwati . Sikuti amafuna kuti tizitsatila ciliconse colembewa m’Cilamulo , koma amafuna kuti tidziŵe na kutsatila “ zinthu zofunika ” kwambili , kapena kuti mfundo zimene panazikiwa malamulowo . Bob anavomeleza , ndipo anacoka panyumba kukacita upainiya ali na zaka 21 . Komabe , pali cinacake cimene cinacitika kuti umoyo wao usinthe . Musaleke kulimbitsa cikhulupililo canu mwa Yehova . Koma pali zambili zofunika monga , amene adzakhala mfumu , amene adzalamulila naye , ndi mmene ulamulilo wao udzakhalila . Komanso magulu ankhondo amene anali kumwamba , anali kumutsatila pamahachi oyela , atavala zovala zapamwamba , zoyela bwino , za mbee ! A Ruth amayi ake , anali Mboni yokangalika mu Wellington , ku Kansas . Iwo anapitiliza kucita upainiya ngakhale atafika zaka za m’ma 90 . 6 : 13 ) Kodi anali makonzedwe otani ? Nanga zimatikhudza bwanji ? MFUMU YOIKIDWA NDI YEHOVA ICITAPO KANTHU Hagara anali wopanda ulemu kwa womulemba nchito wake , Sarai . Cifukwa ca zimenezi , Sarai anamuthamangitsa ndipo Hagara anathaŵila kucipululu . Wapolisiyo anasoŵa coyankha . 24 : 9 . Sitikudziŵa , koma n’zotheka kuti anali ndi nkhawa imeneyo cifukwa cakuti “ anali munthu monga ife tomwe . ” N’cimodzi - modzinso ndi amishonale , atumiki a pa Beteli , oyang’anila dela na azikazi awo , komanso abale amene akutumikila m’maofesi omasulila mabuku . ( Yes . 55 : 11 ) Iye sadzalola kuti kupanduka kwa Satana kusokoneze colinga cake pa mtundu wa anthu . ( 1 Samueli 17 : 57 – 18 : 3 ) Koma Abineri sanakhale bwenzi lake . ( 2 Akor . 6 : 14 ) Malangizo a Mulungu amakhala othandiza nthawi zonse , ndipo Akristu ambili masiku ano asankha kumvela Yehova . Lankhulani mumtima mwanu , muli pabedi panu , ndipo mukhale cete . ” — Sal . Tili na zinthu zabwanji zimene zingalimbitse cikhulupililo cathu ? TSAMBA 8 • NYIMBO : 2 , 75 Kodi abale athu a ku Japan anatengela bwanji citsanzo ca Yesu ? “ Zovala zake ndi zagolide ” ndipo “ adzamubweletsa kwa mfumu atavala covala coluka . ” Tifunika kuyembekezelabe cifukwa comvela Yesu Kristu , ndiponso cifukwa coona cizindikilo ca kukhalapo kwake . Iye anakwatilana ndi mkazi wake wokondedwa Penny mu 1977 , ndipo anali ndi ana . Maziko okha a m’Malemba amene amapatsa munthu ufulu wothetsa cikwati na kukwatilanso kapena kukwatiwanso , ndi cigololo cabe . Ndine amene ndikunena za Koresi kuti , ‘ ‘ Iye ndi m’busa wanga ndipo adzakwanilitsa bwinobwino zonse zimene ndikufuna , ’ ’ ngakhale zimene ndanena zokhudza Yerusalemu zakuti , ‘ ‘ Adzamangidwanso , ’ ’ ndi zokhudza kacisi zakuti , ‘ ‘ Maziko ako adzamangidwa . ’ ” ” Kodi n’zinthu ziti zimene sangakwanitse kucita ? Koma kucokela pamene n’nabwela kuno ku Turkey , nimayamikila Yehova cifukwa ca kuleza mtima kwake . [ 3 ] ( ndime 15 ) Buku ya Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu masamba 52 - 61 , imafotokoza makhalidwe ofunikila kuti tidziphunzitsa mwaluso . Tingatengele bwanji cikhulupililo ca Yobu ? Byron , wa zaka 31 , wa ku Saipan , anati : “ Khama limene akulu amacita mu utumiki ndi kukonda kwao nkhosa , n’zimene zandithandiza kuika patsogolo zinthu za kuuzimu m’malo mofunafuna cuma . ” Patapita nthawi , Yehova anaonetsanso kuti anali kucilikiza gulu lake pamene anayamba kucititsa “ anthu a mitundu ina ” kubwela mumpingo wacikristu . — Ŵelengani Machitidwe 10 : 44 , 45 . Kukamba zoona zimene ndinali kuphunzila m’Baibulo zandithandiza kukhalapo ndi moyo . M’zaka za m’mbuyomu , zofalitsa zathu zinali kupezeka cabe m’Cingelezi . Amuna Odziŵika Bwino 24 : 42 ; Luka 21 : 34 - 36 ) Pa cifukwa cimeneci , tifunika kupitiliza kuyembekezela . Yesu anali kugwilitsila nchito mafanizo pamene anali kulalikila . Munthu aliyense ali ndi ufulu wodziŵa mtundu wa mankhwala amene alipo , ndipo ali ndi ufulu wolandila mankhwala kapena kukana . Mose anapatsidwa malangizo osapita m’mbali omangila cihema , ndi kusankha ansembe . Kodi Akristu ayenela kukondwelela Isitala ? ( Agalatiya 5 : 22 ; Aefeso 2 : 8 ) Mariya anali kucita khama kuti alimbitse cikhulupililo cake . Msilikali akamanga bwino lamba yake , anali kumenya nkhondo molimba mtima podziŵa kuti ni wotetezeka . Kodi Cingelezi cakhudza bwanji nchito ya anthu a Yehova ? Popeleka cilango , muzicita zimenezo moleza mtima ndi mokoma mtima Ngati munthu wina atsutsa cikhulupililo cako pa cilengedwe , mosamala ungam’bwezele nkhaniyo . Blessing ni mmodzi mwa anthu 4 miliyoni amene analoŵapo mu ukapolo wocita malonda a uhule a padziko lonse . Amene analenga cilengedwe conse ndi kupanga dziko lapansi ndi amene analenganso zamoyo zonse . Atate wathu wacifundo cacikulu anavutikapo na cisoni cifukwa ca imfa ya okondedwa ake monga Abulahamu , Isaki , Yakobo , Mose , ndi Mfumu Davide . ( Num . Ngakhale kuti Baibulo linali litagaŵidwa kale kukhala m’macaputala , zikuoneka kuti zinali zovutabe kuligwilitsila nchito . Ngati mwaitanila munthu ku Nyumba ya Ufumu ndipo munthuyo wapezeka , mumakondwela kwambili . N’cifukwa cake Paulo anati : “ Tsopano patsala zitatu izi : Cikhulupililo , ciyembekezo , cikondi . Kodi tifunika kucita ciani kuti tisagwele m’mayeselo ? ( Genesis 40 : 20 ; Maliko 6 : 21 ) Buku yochedwa Encyclopædia Britannica , inakamba kuti Akhristu oyambilila anali kutsutsa “ miyambo yacikunja yokondwelela tsiku lakubadwa . ” Mulungu anapitiliza kukonda anthu . Pamene Uriya anali kunkhondo , Davide anacita cigololo ndi mkazi wa Uriya , Bati - seba , ndipo anakhala ndi pakati . Conde ndiuze . Kodi kunyumba kwa bambo ako kuli malo oti tikhoza kugonako ? ” Onani buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni patsamba 88 mpaka 92 . Pita mu mtendele , matenda ako aakuluwo atheletu . ” — Maliko 5 : 25 - 34 . Kodi makolo amene atumikila mumpingo wa cinenelo cina azindikila ciani ? Pamene musinkhasinkha za citsanzo cake , onani zocitika zisanu pamene anaonetsa cikhulupililo colimba mwa Yehova . Mulungu amasamalila anthu amene amaika zinthu za Ufumu patsogolo mu umoyo wawo . Conco , ife sitifunika kutengela anthu a “ mitundu ina , ” amene alibe cikhulupililo mwa Atate wathu wacikondi wa kumwamba . Nili paulendo wopita kundendeko , n’namvela kuti mwana wathu waciŵili wamkazi Olga , wabadwa . Cifukwa cakuti Yesu amakonda kwambili cilungamo ndipo amadana ndi ciliconse cimene cinganyozetse dzina la Atate wake , Yehova anam’dzoza kukhala Mfumu ya Ufumu wa Mesiya . Sitingakane umboni wakuti anthu ambili anaona Yesu woukitsidwayo . 9 : 37 , 38 ) Tiyeni timve zimene io akufotokoza . 6 : 31 - 33 . Ndinali wamfupi , ndipo ndinali kuvutikabe ndi zinthu zina monga kufikila pa kaunta ya m’sitolo . Ndiyeno , anafotokozela mkazi wake cifukwa cimene ayenela kukomela mtima apongozi ake . * ( 2 Timoteyo 4 : 13 ) Kodi zinthu zimenezi zikanapangitsa bwanji kuti Baibulo iwonongeke ? Mwacitsanzo , mu 1949 , M’bale Grant Suiter ndiye anali mlendo pa msonkhano wacigawo umene unacitikila ku Sioux Falls , m’dela la South Dakota . Tiyeni tione njila zitatu zikulu - zikulu za mmene Baibo ingakhalile yothandiza mu umoyo wanu . Kuti mupeze zitsanzo zina za malangizo othandiza a m’Baibo , onani pa webusaiti ya jw.org , pa cigawo cakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > KUYANKHA MAFUNSO A M’BAIBULO pa webusaiti ya Chichewa . Pamenepa n’zoonekelatu kuti iye anadalitsidwa cifukwa cokhulupilila Yehova Mulungu . Ndipo m’modzi wa mbadwa za Kaini anali wankhanza kwambili ndi wokonda kubwezela kuposa Kainiyo , cakuti anali kucita kunyadila . Woyamba kupatsidwa mphatso imeneyi anali Mwana wake woyamba kubadwa , amene ni “ cifanizilo ca Mulungu wosaonekayo . ” Imeneyo siidzakhala nthawi yolengeza ‘ uthenga wabwino wa Ufumu . ’ Conco , kodi tingati mau a Paulo a pa 1 Akorinto 10 : 13 , atanthauza ciani ? Ngakhale kuti tinakula m’njila zosiyana - siyana , ndife ofanana pa zinthu zina . Ena a inu mumasamalila makolo okalamba olo kuti na imwe ndimwe acikulile . Anthu oona mtima amatonthozedwa akadziŵa kuti Yehova nthawi zonse amacita zinthu mwacilungamo , cifukwa kupanda cilungamo n’kofala m’dzikoli . Masako wa ku Japan amene ali ndi zaka za m’ma 50 , kwa nthawi yaitali anali kulakalaka utumiki waumishonale koma zinali kuoneka kuti ndi zosatheka kaamba ka vuto la thanzi lake . Yehova amakonda kwambili cilengedwe cake . Mwacitsanzo , ganizilani za kagulu ka ofalitsa 25 , kamene kali m’dela lina lakutali m’dzikolo . Ni wogontha mwauzimu . 5 : 11 . Conco , sankhani Baibo imene muli mau osavuta kumva amene angakufikeni pamtima . Ngakhale kuti Marilyn anakaikila zakuti apite kapena ai , iye anatsanzika mwamuna wake James ndi mwana wake Jimmy ndi kupita kukagwila nchito ku dziko lina . Kuyambila m’caka ca 1978 , nthambi ya ku Austria inali kukopa ndi kusindikiza magazini m’zinenelo 6 pa makina aang’ono osindikizila . 4 : 23 , 24 ) Anthu akayamba kuphunzila za Mulungu , amaona kufunika kotsatila mfundo zake pa umoyo wawo . Kodi wamalonda wa m’fanizo la Yesu anali wofunitsitsa kucita ciani kuti agule ngale yamtengo wapatali ? Ndinalimbikitsidwa kwambili ndi nkhani zokhudza umoyo wa Yesu ali pa dziko lapansi . Kodi mumasankha zinthu mwanzelu kuti musasokonezedwe pamene mukuyembekezela ? Komanso imafotokoza zinthu zimene zicititsa ulamulilo wake kukhala wabwino kuposa maulamulilo ena . Kodi Yehova afuna kuti tidziŵe ciani ? Kodi tiyenela kupanga zosankha zotani ? Nanga Mose anatisiila citsanzo cotani ? Cokondweletsa n’cakuti monga Marita , muli na cifukwa cabwino cokambila kuti , ‘ Nidziŵa kuti wokondedwa wanga adzauka pa kuuka kwa akufa . ’ Ndipo kumam’thandiza kuzindikila zimene afunika kuongolela . ” Ena amati kulibe ufulu wosankha zocita . Mulungu anaikilatu zonse zimene timacita . 23 : 22 ) Mabanja amapanga zosankha zosiyana - siyana . TSAMBA 14 Ha , anali mau olimba mtima cotani nanga ! Iye anati : “ Kuchuka , ulemu , mphamvu , na cuma n’zakanthawi cabe ndiponso n’zopanda phindu kweni - kweni mu umoyo . Kucokela pamene n’nabwela ku Wallkill , nauzidwa kuti nathandizapo anthu oposa 600 . Ndani pa zonsezi sadziŵa bwino kuti dzanja la Yehova ndi limene lacita zimenezi ? ” — Yobu 12 : 7 , 9 . Pamene n’nauza asilikali a Greece kuti n’nacita kugwidwa na zigaŵenga , iwo ananitenga n’kukanipeleka ku kampu ya asilikali kuti akanifunse mafunso . Muziyamikila zinthu za kuuzimu Nigeria 330,000 Kodi nimayesetsa kuthandiza ena ? ’ Akakhala na ciyambi cimeneci , amadalitsika potsatila uphungu wakuti kwatilani ‘ kokha mwa Ambuye . ’ Monga “ mlaliki wa cilungamo , ” iye analalikila mokhulupilika uthenga wocenjeza umene anatumidwa . ( 2 Pet . Ngati anthu aloŵa m’cikwati na maganizo aconco , ndiye kuti kungoyambila pa ciyambi , cikwati cawo cimakhala cosalimba . ” — Jean . Yosefe ndi mng’ono wake anali ana aŵili okhawo amene Rakele anabelekela Yakobo . Mwacitsanzo , Asayansi apanga mankhwala a katemela ndiponso mankhwala ogonjetsa matenda enaake . Pamene Aisiraeli anadandaula za utsogoleli wa Mose , Yehova anafunsa kuti : “ Kodi anthu awa apitiliza kundinyoza kufikila liti ? ” ( Num . Nthawi zina tingafunike kufunsa akulu . Kodi nchito yolalikila imayeletsa bwanji dzina la Mulungu ? Kodi timamva bwanji ngati wina ayamikila kupita kwathu patsogolo ? Ngakhale kuti sanali kholo , mungaphunzile kwa iye poona mmene anali kuphunzitsila otsatila ake . Iye anadziona monga kuti wazingidwa ndi mavuto okha - okha . ( Sal . Inde , ngakhale asanam’patse malangizo aliwonse , Yehova anamvetsela kulila kwa mneneli wake ndipo anacitapo kanthu kuti am’thandize . N’ciani cimene atsogoleli a cipembedzo Acikristu anacita panthawi ya nkhondo ? ( Luka 6 : 45 ; 8 : 1 ) Conco , fanizo la Yesu la wofesa mbewu litiphunzitsa kuti malinga ngati tipitiliza kulalikila uthenga wa Ufumu , ndiye kuti ‘ tikubala zipatso mwa kupilila . ’ Nyumba iliyonse imene apezamo anthu ampatuko inafunika kuwonongedwa . ’ Ana athu anali ofunitsitsa kukaonako . Fotokozani mwacidule zimene lemba la Aroma 8 : 15 - 17 limatanthauza . Ngati anthu amene mumadziŵana nawo ali conco , kodi ndiye kuti angakhale mabwenzi abwino ? Zioneka kuti Yesu anakamba mau amenewa m’pemphelo pa nthawi ya ubatizo wake . Kodi Yesu anati “ lamulo lalikulu kwambili komanso loyamba ” ndi liti ? Kodi nyenyezi ndi mapulaneti ndi zoculuka motani ? Nanga zinalengedwa bwanji mwadongosolo ? Mwacitsanzo , mwina mnzathu anatithandiza panthawi imene tinali kufuna kwambili thandizo . Mwacitsanzo , tingadziŵelenga Mau a Mulungu nthawi zonse , koma osazindikila kuti tayamba kukhala ndi mtima wodzikonda . Mu 1998 , nchito ya Mboni za Yehova inavomelezedwa mwalamulo mu Kyrgyzstan . Ngakhale kuti ophunzila ake anali opanda ungwilo , iye anawadalila , ndipo anawauza kuti adzacita nchito zazikulu kuposa iye . Zimenezi zinandikwiitsa kwambili . Mungapindulenso ndi citsanzo ca Petulo pankhani ya zolinga za kuuzimu . Izi zinacititsa kuti akonde kwambili Yehova ndi kuyamba kupita patsogolo kuuzimu . Mu mzinda wa Dublin , munali mwamuna wina wotsutsa kwambili dzina lake O’Connor , amene anali kalembela wa kagulu ka cipembedzo kochedwa YMCA . Aserafi ali na udindo wapamwamba kwambili pakati pa angelo , cifukwa ca utumiki na ulemelelo wawo . Iwo amatumikila ku mpando wacifumu wa Mulungu . — Yesaya 6 : 1 - 3 . ( Salimo 37 : 28 , 29 ) Baibo imalonjeza kuti posacedwapa Mulungu adzathetselatu zinthu zoipa . — Ŵelengani 2 Petulo 3 : 7 - 9 , 13 . ( Miyambo 26 : 14 ) Mwanjila imeneyi , nchito imathandiza munthu kukhala wosangalala . Kodi n’ciani cingatilepheletse kukhalabe ndi maganizo oyenela ? Iye amafika posintha umoyo wake , kaganizidwe kake , ndi zocita zake . Makolo anga a William ndi a Jean anali kulambila Yehova modzipeleka . Mvelani zimene zinacitikila mlongo wina dzina lake Tessie , amene amakhala ku Australia . Komabe , kudziŵa dzina la Mulungu lakuti Yehova , kwathandiza anthu ambili a mitima yabwino kuyandikila Mulungu . Kwina kumene apainiya nthawi zambili anali kufikila akapita ku Dublin , kunali kunyumba kwa Ma Rutland , mlongo wokhulupilika amene anali ciyambakale m’coonadi . Imililani mowongoka M’malo mwake , ‘ Sara anali womvela kwa Abulahamu , ndipo anamucha kuti “ mbuyanga . ” ’ ( 1 Pet . Nanga zinthu zinawayendela bwanji ? Maganizo athu : Kuti tikhale ndi khalidwe labwino , tiyenela kukhala ndi maganizo oyenela . Nthawi zina , munthu wokonda zinthu zakuthupi sakhala cabe munthu wandalama zambili kapena katundu wodula . Muziona zinthu zotheka . N’ciani cingatithandize kukaniza ‘ zosangalatsa zosakhalitsa zaucimo ’ ? Pa 27 April , mu 1986 , ananibatiza mwakabisila m’bafa yosambilamo , cifukwa panthawiyo Mboni zinali zoletsedwa ku East Germany . N’cifukwa ciani Yesu anafotokoza fanizo la khoka ? Limeneli ndi limodzi mwa mavesi odziŵika kwambili ndiponso limene anthu nthawi zambili amagwila mau m’Baibulo . Monga mmene Baibo imakambila , “ mtendele wa Mulungu ” unali ‘ kuteteza mtima wanga ndi maganizo anga . ’ ( Afil . Koma Mkhristu safunika kucita zimenezi . N’cifukwa ciani pali zimasulilo zambili zosiyana - siyana za Baibo masiku ano ? M’caka ca 1914 cabe , Ophunzila Baibo ocepawo anatambitsa “ Seŵelo la Pakanema la Cilengedwe ” kwa anthu oposa 9,000,000 . Ndinabatizidwa mu July 1971 , pa msonkhano wacigawo wa mutu wakuti “ Dzina la Mulungu , ” ku Yankee Stadium Kodi mungawonjezele zocita pa nchito imeneyi ? — 1 Tim . Yesu anaseŵenzetsa mau amenewo pokamba na mkazi amene anali na matenda otaya magazi kwa zaka 12 . N’zoona kuti Mulungu analonjeza kuti adzapatsa atumiki ake okhulupilika zinthu zofunikila pa umoyo wao . Wamasalimo amene anali kukonda kwambili Yehova ndi kum’dalila analemba kuti : “ Yembekezela Mulungu , ndipo ndidzamutamanda pakuti iye ndiye mpulumutsi wanga wamkulu . ( Aroma 12 :⁠ 2 ) N’cifukwa ciani kucita zimenezi n’kofunika ? Kodi Baibo imakambanji ponena za kaimidwe kawo ka maganizo , mmene anali kumvelela , komanso kacitidwe kawo ka zinthu ? Ndipo anayamba kulambila mafano pamodzi ndi azikazi ake . Ngati tifuna kuti Yehova azikondwela pamene tim’tumikila , tiyenela kudzipeleka kwa iye yekha ndi kum’konda ndi mtima wathu wonse , maganizo athu onse , ndi mphamvu zathu zonse . 8 - 10 . ( a ) Kodi lemba la 2 Timoteyo 3 : 1 - 5 likukwanilitsidwa motani ? [ Mau apansi ] A Mboni za Yehova ali ndi njila yabwino imene amatsatila pokambilana Baibulo ndi anthu kwaulele pa nkhani zosiyanasiyana . Yesu analonjeza kuti Atate wathu wakumwamba sadzalephela kupatsa mzimu woyela anthu omupempha . N’cifukwa ciani Paulo anauza Timoteyo kuti “ thaŵa zilakolako zaunyamata ” ? Iwo anakhala m’dzikolo mpaka pamene Herode anamwalila . YEHOVA amakondwela kugwila nchito . ( Sal . 135 : 6 ; Yoh . Kuzindikila kunathandizanso Yesu kuganizila ena . Hans atapika ndende zaka 17 na hafu , anatulutsidwa ndipo panthawiyo anali atabatizika monga Mboni . Pambuyo pake , n’naganiza zoyamba upainiya . Buku lina linati , “ Ubatizo ndi wofunika kuti munthu akapulumuke . M’pake kuti buku lakuti The World Book Encyclopedia limati : “ Malamulo a m’dziko lililonse amapanga msakanizo wovuta kumvetsa wa maufulu ambili na ziletso zake . ” Komanso mlongo Julia Wilcox analemba kuti : “ Siningakwanitse kufotokoza cimwemwe cimene nimakhala naco nthawi iliyonse ngati m’mabuku athu akambamo za msonkhano umene unacitika ku Cedar Point mu 1922 . Ngakhale kuti ena amacita mantha ndi masomphenya a amuna anayi okwela pa mahosi , sikuti colinga cake ni kukuwopsezani . Mtsikana wina wa zaka 18 , anati : “ Mwana amene ni wa Mboni za Yehova sangakhumudwe ngati anzake ku sukulu sanam’patseko keke ya pa mwambo wokumbukila tsiku la kubadwa . Cinsinsi Namba 4 Kukhululukilana Ngakhale kuti m’kupita kwa nthawi Sauli anaphedwa ku nkhondo , Davide anafunika kuyembekezelabe kwa zaka zina 7 kuti aikidwe kukhala mfumu ya mtundu wonse wa Isiraeli . — 2 Sam . NYIMBO : 48 , 95 Ndinayamba kudwala pamene ndinali kugwila nchito m’cipinda cocitila opaleshoni panthawi ya nkhondo ku Vietnam . Ganizilani za Sara , mkazi wa Abulahamu . 2 : 21 . 17 , 18 . ( a ) N’cifukwa ciani Sinara anali ‘ malo oyenela ’ kukhalako ‘ zoipa ’ ? Ngati Yehova sakanatikonda , tsogolo lathu likanakhala loipa kwambili . N’cifukwa ciani Yehova analola anthu kupandukila ulamulilo wake ? 4 , 5 . ( a ) N’ciani cimatithandiza kumvetsa bwino lemba la Aroma 5 : 12 ? A Inoki : Ndakondwela kumva zimenezi a Yohane . Pamene Satana ndi anthu aŵili oyambilila anapandukila ulamulilo wa Yehova , iwo anacita zinthu modzikuza . 28 : 19 ) N’zotheka kukwanilitsa nchito imeneyi ndi thandizo la Yehova Mulungu . Umboni wa zimenezi ndi wakuti iye anacha guwa la nsembe limene anamanga pamalowo kuti “ Yehova - salomu . ” Kodi tingapeleke fanizo lotani kuti tionetse kuti Mulungu ndi wamkulu kuposa Yesu ? ▪ Mosiyana ndi anthu amene amalosela kuti dziko lidzaonongedwa , Mulungu amatitsimikizila kuti Dziko Lapansi silizaonongedwa . — Salimo 104 : 5 ; Mlaliki 1 : 4 . Atalimbikitsidwa ndi citsanzo ca apainiyawo , Tatyana akakhala pa holide anali kupita ndi ena ku magawo akutali a ku Ukraine ndi Belarus kumene Mboni sizinalalikileko . N’cifukwa ciani kukopana n’koopsa ? Koma ine ndikukuuzani kuti : Pitilizani kukonda adani anu ndi kupemphelela amene akukuzunzani , kuti musonyeze kuti ndinudi ana a Atate wanu wakumwamba . ” N’zoona kuti colinga ca funsoli n’cakuti tidziŵe maganizo a mwininyumbayo kuti tiyambitse makambilano a m’Baibulo . Kope ino ya Nsanja ya Mlonda ipeleka umboni woonetsa kuti Baibo ingatithandize m’mbali zonse za umoyo wathu . Mtumwi Paulo analembela Akhiristu aciheberi kuti : “ Munapilila mayeselo aakulu ndi masautso . ” Iwo anacita izi pofuna kuti Yehova awayanje ndi kuwadalitsa . Mu 1995 , mpingo woyamba unakhazikitsidwa m’tauni ya Balykchy . Izi zinacitika patapita zaka 8 kucokela pa ulendo woyamba umene tinapita kukalalikila m’tauniyo . Kodi alimiwo anamulandila mwanayo ? M’zaka zocepa cabe , kunakhazikitsidwa mipingo 8 . 14 : 28 ) Ndiyeno tingam’funse kuti : “ Kodi anthu aŵili a m’banja limodzi angakhale olingana ngati ali paubale wotani ? ” Koma m’kupita kwa nthawi , anakhutila kuti Mulungu amam’kondadi . Atatulutsidwa mu ukapolo ku Iguputo , anthu a Mulungu anafunika kulandila malangizo atsopano . ( Yoh . 6 : 44 ; 14 : 6 ) Motelo , Yehova amakoka anthu kupyolela mwa Yesu , ndipo amawathandiza kukhalabe m’cikondi cake kuti akalandile moyo wosatha . Ndipo zikadzakala conco , Ayuda mamiliyoni ambili amene anabalalikila m’maiko ena adzabwelelanso m’dziko lawo . Kukamba zoona , kukhala moyo wosafuna zinthu zambili kudzatithandiza kuti ‘ tigwile mwamphamvu moyo weniweniwo ’ umene uli m’njila . — 1 Tim . 13 : 7 . Zimenezi zathandiza kuti zofalitsa zathu zizimasulilidwa bwino kwambili . Mwina mungadabwe kuti , ‘ N’cifukwa ciani m’mipingo ya Mboni za Yehova munali tsankho ? ’ Mulungu watipatsa mwayi wothandiza acatsopano kuti akwanitse kutumikila bwino mumpingo . Mmene anali kucitila zinthu . Mwacitsanzo , iye amatiuza kuti sitiyenela kulambila mafano , kuba , kuledzela , kapena kucita ciwelewele . Musandibisile nkhope yanu . ” Mwacitsanzo , bwana wa pa kampani ina yaikulu atapita kukaona makina athu opulintila , anadabwa kudziŵa kuti nchito yonse imagwilidwa na anchito ongodzipeleka . Anadabwanso kudziŵa kuti siticita malonda , koma timaseŵenzetsa cabe ndalama zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo . Atumiki a Yehova padziko lapansi akhala akupindula akamaganizila mmene malonjezo a Mulungu adzakwanilitsidwila . “ Yehova Ndiye Mwini Nkhondo ” ( Davide ) , Na . ( a ) Kodi kukamba ndi wophunzila nkhani ya zolinga za kuuzimu kuli ndi ubwino wotani ? Anthu ena akamaganizila za tsogolo lao , amakhala ndi nkhawa kwambili . Maloto oyambilila analota kuti , iye ndi abale ake akumanga mitolo ya tiligu . Kukamba zoona , anthu amayamikila a Mboni za Yehova cifukwa ‘ amadzikongoletsa ndi zovala zoyenela , povala mwaulemu ndi mwanzelu . . . mogwilizana ndi mmene akazi amene amati amalemekeza Mulungu amayenela kudzikongoletsela . ’ ( 1 Tim . 2 : 9 , 10 ) Apa mtumwi Paulo anali kukamba za akazi . Ofesi ya nthambi imene tinacezela inakumana ndi vuto lalikulu , ndipo abale a m’Komiti ya Nthambi anacita zimene akanakwanitsa kuti athetse vutolo . Mkulu wina amene akutumikila pa ofesi ya nthambi ndipo amalankhula ndi apainiya apadela ambili anati : “ Akulu ayenela kulankhula nao , kudziŵa mmene zinthu zilili paumoyo wao , ndi kuona mmene angawathandizile . ( Yoh . 1 : 12 , 13 ; 3 : 5 - 7 ) Cifukwa codzozedwa ndi mzimu woyela , anthu amenewa amachedwa “ ana a Mulungu . ” ( Aroma 12 : 15 ) Gaby , amene mwamuna wake anamwalila , anati : “ Kulila n’kumene kumanitonthoza . Kodi amafuna kutilanga tikangolakwitsa zinthu ? Bukulo linanena kuti “ anali kuzithila mcele wamiyala kuyambila mopumila mwake , kukamwa ndi m’mamba ake . Nthawi zonse tinali kulalikila kunyumba ndi nyumba pamodzi monga banja . — Mac . 20 : 20 . Conco ngakhale kuti zofalitsa zimenezi analembela acinyamata , uthenga umene ulimo umacokela m’Baibulo , ndipo ungapindulitse Akristu onse . Kodi Yehova adzacita ciani cimene cidzatsogolela ku Aramagedo ? Koma mkupita kwa nthawi , anthu ambili amene anali kuyembezela kudzakhala padziko lapansi anayamba kudzigwilizanitsa ndi Ayuda auzimu . ( Zek . 1 , 2 . ( a ) Kodi Yesu anapempha ciani m’pemphelo lake lothela limene anapeleka ali na atumwi ake ? Kodi zocita za anthu oipa zimatikhudza bwanji masiku ano ? Kodi Yesu akucita ciani tsopano ? Nanga pamenepa pabuka mafunso otani ? Ganizilani zimene mwaphunzila , ndipo onetsetsani kuti mwazimvetsetsa . Ni mavuto ati amene timakumana nawo ? Nanga n’cifukwa ciani Yehova amakondwela na atumiki ake okhulupilika ? Kodi m’bale wina anati ciani za kusiyila ena maudindo ? ( Maliko 12 : 30 ) Yehova amafuna kuti tizim’konda ndi ‘ mtima wonse . ’ Kupezeka pa Cikumbutso kudzakuthandizani kusinkhasinkha pa ciyembekezo canu ndi kuona kuti imfa ya Yesu ndi yofunika kwambili . Anaoloka nyanjayo onse pamodzi monga gulu motetezedwa ndi Yehova . Zinali kundivuta kucilikiza cisanduliko . ( b ) Nanga io amapeleka citsanzo cotani kwa ife ? Ndiyeno anathamangila m’bwalo la nkhondo . Imatithandiza kugwilitsila nchito malangizo ocokela ku Bungwe Lolamulila . Cifukwa Cake Tifunika Kukhala Oyela ( 1 Ates . 2 : 2 ) Kodi ise tingaonetse bwanji kuti timakonda ulaliki ? M’nkhani ino ndi yotsatila , tikambilana pemphelo lacitsanzo . Riana anati : “ Atate anga , amalume , na ambuya aakazi , onse anali kunilimbikitsa kuti nikacite maphunzilo apamwamba . Kodi tingacotse bwanji tsankho m’mitima yathu ? Kodi nchito yolalikila imatiteteza bwanji ? Ali na zaka 90 , Sara anakondwela kwambili kuona kuti zimene anali kulaka - laka mu umoyo wake zacitika . Ali wacinyamata , Timoteyo anadzipeleka kuyamba utumiki wacikristu N’cifukwa ciani dipo imene Mulungu anapeleka imaonetsa cisomo cake ? ( Mat . 9 : 35 ; Luka 9 : 11 ) Kunena zoona , Yesu anaonetsadi mphamvu za Mulungu . Tikasiliza kuphunzila Baibulo , ophunzila ena , anali kutitsatila tikapita pa nyumba ina n’colinga cakuti akaphunzilenso . M’kupita kwa nthawi , m’ndandanda umenewu unakhala dikishonale . Kodi cinathandiza Ana kupilila n’ciani ? Cakumapeto kwa zaka za m’ma 1800 , kodi Akristu oona anapatsidwa cizindikilo cotani ? ( Mat . 22 : 37 , 38 ) Ndithudi , kukonda kwambili Mulungu kumatithandiza kumvela malamulo ake , kupilila , ndi kudana n’zoipa . ( 1 Yohane 3 : 8 ) Anthu mamiliyoni ambili masiku ano amapemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele . Yesu anaika maganizo ake pa madalitso amene anali kudzalandila cifukwa ca kupilila kwake Munthu wina dzina lake Ulf , amene poyamba anali na thanzi labwino , anazizila ziwalo . Iye anati : “ N’navutika maganizo kwambili . Dzina lakuti Zekariya , limene limatanthauza kuti “ Yehova Wakumbukila , ” liyenela kuti linawakumbutsa mfundo yofunika kwambili . Yesu anakamba kuti anamwali 10 “ onse anayamba kuwodzela kenako anagona ” pamene anaona kuti mkwati akucedwa . Tiyenela kuyamikila ndi kupemphelela amene amakwanilitsa udindo wao wosamalila banja popanda kusiya mkazi ndi ana , ngakhale kuti ena angawakakamize kuti acite zimenezo . Mu April 1911 , Ophunzila Baibo 20 a ku Belfast analandila alendo 2,000 amene anabwela kudzamvetsela nkhani yakuti “ Moyo Pambuyo pa Imfa . ” Nanga n’ciani cimene atumwiwo anafunika kucita kuti akhalebe mabwenzi ake ? “ Onse pamodzi anafuula kwa Mulungu mokweza mau , ” ndi kupemphela kuti apitilize kuwathandiza “ m’dzina la Yesu , mtumiki [ wake ] woyela . ” Nanga n’cifukwa ciani Mose anawakumbutsa kuti Yehova Mulungu wawo ni “ Yehova mmodzi ” ? Mwacitsanzo , lipoti ina yaposacedwa inakamba kuti anthu olemela kwambili , amene ciŵelengelo cawo cikwana cabe 1 pelesenti ya anthu onse padziko , ali na cuma colingana ndi ca anthu onse padziko lapansi tikaciphatikiza pamodzi . N’zoona kuti anthu ena angakayikile zimenezi . Conco , dzifunseni kuti , ‘ Kodi moyo wanga nidzaugwilitsila nchito bwanji ? ’ Limeneli linali vuto lalikulu , maka - maka tikakumbukila mau a Yesu akuti : “ Aliyense wovomeleza pamaso pa anthu kuti ali kumbali yanga , inenso ndidzavomeleza pamaso pa Atate wanga wakumwamba kuti ndili kumbali yake . Mwamuna amene anataya ndalamazo ndi banja lake anadadwa kwambili . Tsiku lina m’maŵa mu April 1908 , abale 5 anamulandila atafika pa doko la ku Belfast . M’madela ambili anthu amaona kuti ali ndi udindo wopatsa acibale ndi mabwenzi ao ndalama ndi mphatso . Dzina limeneli limatanthauza kuti “ Yehova Ndiye Mlongoti Womwe Ndi Cizindikilo Canga . ” — Ŵelengani Ekisodo 17 : 14 , 15 ; mau a munsi . Koma cifukwa conyalanyaza , mkulu wa opelekela cikho anaiŵala zimene Yosefe anamuuza . — Genesis 40 : 20 - 23 . ( Yohane 15 : 19 ; 17 : 16 ) Pa nkhondo yaciŵili ya padziko lonse , Mboni za Yehova zinaikidwa m’ndende , kuzunzidwa ndi kuphedwa cifukwa cokana kuloŵelela m’ndale za dziko . N’cifukwa ciani timachedwa mabwenzi a Yehova ndiponso “ anchito anzake ” ? 23 : 2 . ( Ŵelengani Miyambo 16 : 32 ; Mlaliki 7 : 9 . ) Munthu amene amakukondani akadziŵa kuti mukufuna kuleka sukulu angakuthandizeni kuzindikila kuti sukulu idzakuthandizani kukhala munthu wakhama pocita zinthu . Khalidwe limeneli n’lofunika kwambili ngati mufuna kutumikila Yehova kwamuyaya . — Sal . 4 : 6 , 7 ) Ngati nthawi zonse timapemphela na kudalila mzimu wa Yehova , iye adzatipatsa mtendele woculuka umene umakhala cabe ndi anthu amene ali pa ubwenzi wabwino na iye . — Aroma 15 : 13 . Baibulo limati : “ Munthu akakhala pa mayeselo asamanene kuti : ‘ Mulungu akundiyesa . ’ ” Amakhala opatsa Kumbukilani mwambi wouzilidwa uwu : “ Munthu woyenda ndi anthu anzelu adzakhala wanzelu , koma wocita zinthu ndi anthu opusa adzapeza mavuto . ” ( Miy . Mau amenewa aonetsa kuti Yesu anasintha nkhani . Poyamba , umoyo wa m’ndende sunamuthandize Hans kusintha khalidwe lake laciwawa . Fotokozani mmene Yehova anathandizila amuna ena aciisiraeli kutsogolela anthu ake . Mwacitsanzo , cioneka kuti Yosefe , atate ake a Yesu omulela , anafa iye akali wacicepele . Buku limodzi lokha limene linapo m’cinenelo cimeneci linali buku la “ New Testament . ” ( Ŵelengani Nyimbo ya Solomo 1 : 2 , 3 . ) Cakudya cakuuzimu cimene Yehova amatipatsa ciphatikizapo Baibulo , zofalitsa zopulintidwa , ndi zimene zimapezeka pa jw.org . Kupepesa kungathandize kuthetsa mkwiyo , koma sikufunika kukhala kwaciphamaso . Kodi mungatani kuti mudzapulumuke ndi ‘ kukhala kosatha ’ pamene dzikoli lizidzaonongedwa ? Tonse tinalila . 21 : 12 , 13 . Mwacitsanzo , Asuri ataopseza kuti adzaononga Yerusalemu , Hezekiya anasonkhanitsa akulu - akulu a asilikali ndi anthu a mu Yerusalemu kuti awalimbikitse . Nanga tingacite bwanji zimenezi ? ‘ Usamadzitopetse ndi nchito kuti upeze cuma . Popeza kuti mlongoyo anali kudziŵa kukamba citundu ca John ca Cigujarati , anamuyankha poseŵenzetsa Baibo , ndipo anam’patsa kabuku kakuti , “ This Good News of the Kingdom , ” ( “ Uthenga Uwu Wabwino wa Ufumu ” ) . Yehova afuna kuti inuyo mudzakhale na umoyo wotelo . Yehova anali kufuna kuti io azikhala ofunitsitsa kuthandiza osauka . — Deut . Coyamba io anali kutenga nsombazo n’kuzitumbula kenako n’kuzitsuka ndi madzi . Mwa ici , n’nayamba kuganizila mau a Yesu , akuti tiyenela ‘ kuunjika cuma kumwamba . ’ Iye ananiyankha kuti , “ Ufuna nicite ciani ? ” Malangizo amenewa anali oŵaŵa , koma ndi amene ananithandiza . Iye sanamvetse cifukwa cimene Yonatani anali kukondela Davide . Kodi zosankha zanga zidzanithandiza kupita patsogolo mwauzimu ? ndipo mphepoyo ikuleka . Kodi cikumbumtima cathu cingatithandize bwanji posankha . . . N’zacisoni kuti nthawi zina timaŵelenga zinthu popanda kuziganizila . Mlongo Kumiko , wa zaka za m’ma 60 , anali mpainiya wathawi zonse ku Japan . Ali kumeneko , mpainiya mnzake anam’pempha kuti asamukile ku Nepal . Nthawi ina pamene anali m’cipatala , analalikila kwa maola 80 , m’mawiki yaŵili na hafu cabe . Ulamulilo wake udzakhalapo mpaka kalekale ndipo sudzatha . Ufumu wake sudzawonongedwa . ’ — Danieli 7 : 14 . Ŵelengani Salimo 45 : 1 . Mumam’lonjeza kuti kumutumikila kudzakhala cinthu cofunika kwambili pa umoyo wanu . Farao ndi atumiki ake anaona kuti zimene Yosefe anakamba n’zanzelu . M’bale wina amene anapeza cimwemwe potumikila ena ndi Ramiro . Iye anauza Aisiraeli akale kuti : “ Mukhale oyela , cifukwa ine Yehova Mulungu wanu ndine woyela . ” 17 : 5 , 6 . 6 , 7 . ( a ) Ponena za kukhala mutu wa banja , kodi Baibulo limakamba ciani ? Makhadi a ulaliki anathandiza ofalitsa m’njila zosiyanasiyana . Komabe , buku yakuti Encyclopædia Britannica inakamba kuti podzafika “ ca kumapeto kwa zaka za m’ma 900 , azibusa ambili ngakhale mabishopu ena anali ndi akazi . ” Mfumu ina imene inalamulila Aisiraeli kwa zaka 40 inatamanda Mulungu ndi mau akuti : “ Yehova ndi wacifundo ndi wacisomo , Wosakwiya msanga ndiponso wodzaza ndi kukoma mtima kosatha . Mwa ici , sakhala odzicepetsa . ( a ) Tingagwilitsile nchito motani lemba la Miyambo 30 : 4 kuphunzitsa munthu za dzina la Mulungu ? Mwacitsanzo , Mulungu anafuna kuononga Aisiraeli pamene anapanga fano la mwana wa ng’ombe wa golide , koma Mose atamucondelela , iye anasintha maganizo Ake . — Eks . Anthu anacita cidwi ndi mmene buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu linalembedwela . ( Yak . 3 : 2 , 5 , 8 ) Okwatilana ambili amagwila nchito yopanikiza kwambili komanso kusamalila ana . 3 : 7 . Khama n’lofunika kuti tizisinkhasinkha ndi kuika maganizo pa zimene tiphunzila . Tinayesetsa kumusamalila bwino mmene tikanathela , kwinaku tikusamalilanso ana athu ena 4 . Adzakhuthulila m’matumba anu muyezo wabwino , wotsendeleka , wokhuchumuka ndi wosefukila . Makolo okalamba a abalewa anafunikila cithandizo . Psarras ) , Apr . M’zaka za m’ma 200 zoyambilila , mwambo wa kusakwatila m’pamene unayamba kutenga malo m’machechi “ Acikhristu ” m’maiko a azungu . Kodi cidzacitika n’ciani Gogi wa Magogi akadzayamba kuukila anthu a Mulungu ? N’ciani cimene munthu afunika kucita kuti athetse vuto la kutamba zamalisece ? Kodi mukumva bwanji kukhala ndi kamvedwe katsopano kokhudza lemba la Mateyu 24 : 45 - 47 ? ( Chiv . 6 : 2 ) Anayeletsa kumwamba pankhondo yake yolimbana ndi Satana ndi ziwanda zake , amene anaponyedwa padziko lapansi . M’nthawi ya Aisiraeli , Yehova anali kuona mlandu uliwonse wa kupha munthu kukhala nkhani yaikulu kwambili . M’dzikolo munali amuna ndi akazi ambili , ndipo onse anali athanzi ndi amphamvu . “ Pakuti Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha , kuti aliyense wokhulupilila iye asawonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” — Yohane 3 : 16 . Koma zinthu zimenezo zinali zosakhalitsa . Ngati mufuna kudziŵa za Mulungu , tikukulimbikitsani kupempha wa Mboni za Yehova kuti akuthandizeni kuphunzila Baibulo . N’cifukwa ciani tiyenela kulola Yehova kuti atitsogolele tisanapange zosankha ? N’ciani cingathandize ? “ MULUNGU ndiye mzimu , ” ndipo anthu sangathe kumuona . Pa nkhani ya mgwilizano , kodi Yehova anamuuza ciani Ezekieli ? ( Ŵelengani Mateyu 23 : 10 . ) * Komanso Mulungu sanaulule ngakhale dzina lolongosola zocita za mdani ameneyu , mpaka patapita zaka 2,500 kucokela pamene iye anapanduka mu Edeni . N’cifukwa ciani muyenela kucita cidwi ndi mmene maulosi a Mulungu anakwanilitsidwila m’nthawi zakale ? ( Yohane 11 : 25 , 26 ; 17 : 3 ) Pamene ophunzila ake 70 anabweletsa lipoti la mmene nchito yolalikila inayendela , iye “ anakondwela kwambili ” na kufuula kuti : “ Kondwelani cifukwa mayina anu alembedwa kumwamba . ” — Luka 10 : 20 , 21 . Kodi tingalimbitse bwanji cikhulupililo ca abale othaŵa kwawo akangofika m’dela lathu ? Iwo amakonda kufotokozela ena mumpingo mfundo za m’Baibo . Ngati cikumbumtima ca munthu si cophunzitsidwa bwino , sicingamuletse kucita zoipa . ( 1 Tim . ( 1 Yohane 4 : 8 ) N’cifukwa cake m’pake kuti Yehova amachedwa “ Mulungu wacimwemwe . ” Nanga mungathandize bwanji aja amene ali mu utumiki wanthawi zonse ? N’cifukwa ciani Paulo ayenela kuti zinam’dabwitsa ataikidwa m’ndende ? Patapita zaka zocepa , Livija anaikidwa kukhala mpainiya wapadela . Kodi akufuna ciani ? Kodi Baibo imaonetsa kuti cilango n’cinthu cotani ? Koma palibe amene angatsutse kuti anthu mabiliyoni ali pa umphawi wosaneneka , ngakhale kuti ampondamatiki ena ali na cuma coculuka kwambili cimene iwo , ana awo , ndi azidzukulu awo angacigwilitsile nchito koma osacitsiliza . Zimenezi zimacitika kwambili ngati boma ndilo limayang’anila ofalitsa nkhani . Yehova amaseŵenzetsa nsembe ya Khiristu kuti akhululukile macimo a anthu amene amaonetsa cikhulupililo . Angotsala pang’ono kundiponya miyala ! ” Iwo anali kudzifunsa kuti : ‘ Kodi Maria ni wamkulu mokwanila cakuti n’kubatizika ? 3 : 1 - 6 ) Kodi kupanduka kumeneku kumawakhudza bwanji akazi ? Zimene Abele anali kudziŵa zokhudza colinga ca Mulungu zinamuthandiza kukhala ndi ciyembekezo ca tsogolo labwino ndiponso cikhulupililo . Ngakhale mlili wocokela ku makoswe sunaphe anthu oculuka cotelo pa nthawi yocepa . ” N’cifukwa ciani amaŵaona kuti ndi odetsedwa ngakhale kuti io ndi munthu wabwino ? Posacedwapa , anthu amene amakana ulamulilo wa Yehova adzacotsedwa pakati pa anthu a Mulungu . Mofanana ndi mmene Mulungu amaphunzitsila , citsanzo canu makolo , cingathandize pophunzitsa ana anu kukonda Mulungu .⁠ — Ŵelengani Deuteronomo 6 : ​ 5 - 7 ; Aefeso 4 : ​ 32 ; 5 :⁠ 1 . Nanga anthu amene amakhala na mbali yophunzitsa ena mumpingo , angaonetse bwanji kuti Malemba ndiwo maziko a zimene amaphunzitsa ? Aroma asanayambe kugwilitsila nchito phula popanga ngalawa zao kuti madzi asaziloŵa , Aakediya ndi Ababulo akalekale anali atayamba kale kucita zimenezi . Nthawi zina nimafika ku Nyumba ya Ufumu ndili wosakondwa . Palibe zifukwa zomveka zokayikilila nkhani imeneyi . Anafunikila kukhalabe okhulupilika kuti akapite kumwamba kukalamulila pamodzi na Khiristu . Ngati umunthu wanu muudziŵa bwino , mudzakwanitsa kukhalila kumbuyo zimene mumakhulupilila , komanso kupewa kumangotengela zocita za anzanu . Mnyamatayo anali patsogolo ndipo anateleleka ndi kugwela pamadzi osefukilawo kaŵili konse . 4 : 3 - 6 ) Ni kangati pamene anthu amakuyankhani kuti “ Sinifuna ” mukafuna kuwalalikila ? Nditafika zaka 10 , ndinayamba kutumikila mahule ndi anthu amene anali kucita katapila kapena kuti kukongoza ndalama zakaloŵa . Iye anali atatsala pang’ono kufa monga nsembe ndi kusonyeza kuti Mdyelekezi ndi wabodza . Iwo anali kubwela kudzacita zinthu zowathandiza kukhala na moyo wathanzi , koma anali kubwelela kwawo ali na ciyembekezo ca moyo wosatha . N’cifukwa cakuti panali kusagwilizana pankhani yokhudza Mulungu mumgwilizano wao . “ Iye anakuuza zimene zili zabwino . ( Mac . 23 : 6 - 9 ) Anthu ena anali kudana ndi okhometsa msonkho . ( Mat . 9 : 11 ) Ndipo anthu odziŵa cilamulo anali kuona anthu osadziŵa Cilamulo kukhala otembeleledwa . Colinga cathu cizikhala kupewa macimo akulu - akulu , pamodzi na zolakwa zing’ono - zing’ono . Conco , tonse tili na mbali zina zofunika kuwongolela kuti tikulitse khalidwe la cikondi . Leka kufunafuna njila yomasukila . ” Mwacitsanzo , Abulamu “ anasonkhanitsa anyamata ake odziŵa kumenya nkhondo ” kuti akapulumutse Loti , ndipo anyamatawo anapambana . 5 , 6 . ( a ) Pelekani zitsanzo zoonetsa kuti angelo ndi “ amphamvu . ” ( b ) N’cifukwa ciani tinganene kuti Satana ali ndi “ njila yobweletsela imfa ” ? Cilungamo ni mbali ya umunthu wake , ndipo malamulo amene iye anapatsa anthu ni ogwilizana ndi cilungamo cakeco . Iye anati : “ Kwa inu nonse amene mungakwanitse kutumikila kosoŵa , nikukulimbikitsani kuti mucite zimenezo . 5 : 11 , 12 ; 91 : 14 . 3 Mphatso Yosangalatsa ya Anthu a ku Japan M’nkhani ino tidzaphunzila cifukwa cake anthu ambili amakhulupilila kuti Mboni za Yehova zili ndi coonadi . Iwo sanakayikile ngakhale pang’ono kuti Yehova anayankha mapemphelo awo . Kodi Yehova anapeleka ciweluzo cotani pa nkhaniyi ? Nanga n’cifukwa ciani anam’tsekela m’menemo ? Iye anaonjezela kuti : “ Ndimasamba ndi kumeta ndevu tsiku lililonse . ” Olo zinali conco , kupilila kwathu kunabala zipatso . Amaopa kuti nchitoyo sidzayenda bwino . 27 : 11 ) Lelo linonso , makolo ambili acikhiristu , amadzipeza mu mkhalidwe umenewo . Margaret anaiŵala kuikamo makaloni , amene ndiye cinali cakudya ceni - ceni ! Kucita izi sikutanthauza kuti timaona cipulumutso cathu kukhala cosafunika , kapena kuti timadziona ngati osafunika pamaso pa Mulungu . Mfundo ina ya m’Baibo imati : “ Ngati ndi kotheka , khalani mwamtendele ndi anthu onse , monga mmene mungathele . ” Zida zothandiza pophunzila Baibo zingakuthandizeni kumvetsetsa zimene muŵelenga . Pamenepo Mose anatenga magaziwo [ a ng’ombe zazimuna ] ndi kuwaza anthuwo , ndipo anati : ‘ Awa ndiwo magazi okhazikitsila pangano limene Yehova wapangana nanu mwa mau onsewa . ’ ” — Eks . Mariya Mu 2012 , iwo anayenda ku Ghana ndipo anatumikilako miyezi 4 . Kumeneko anali kucilikiza mpingo wa cinenelo ca manja . Iye anati : “ Ine na mkazi wanga tinali na mtendele wa m’maganizo umene lemba la Afilipi 4 : 6 , 7 limakamba . Nchito imene iwo amagwila ni imene ine n’kanagwila nikanaphunzila za malamulo . Tidziŵa kuti Yehova amayamikila kwambili zonse zimene amacita mocokela pansi pamtima . 8 : 10 . Kodi anthu adzafika poliwonongelatu dziko lapansi ? Pamene ndapita kumaiko osiyanasiyana , ndatsimikiza kuti Mboni za Yehova n’zogwilizana padziko lonse lapansi . Kodi pemphelo limathandiza bwanji ? ( Mateyu 11 : 19 ) Mogwilizana na mfundo imeneyi , kukhala wokhutila , ndi wopatsa , komanso kuona anthu kukhala ofunika kuposa zinthu , ndiye zimathandiza munthu kukhala wacimwemwe . William anati : “ Vuto lalikulu limene tinali nalo ndi kusiya umoyo wosasoŵa kanthu . ” ( Ŵelengani Mateyu 22 : 37 , 38 . ) Yehova anawapatsanso zocita . ( Num . 7 : 89 ; Ezek . Mau amenewo anandilimbikitsa kwambili . ” Mukakhala na nkhawa yaikulu , mantha , ndi cisoni , n’ciani cingakuthandizeni kukonzekela za kutsogolo ? Anthu ena oipa angaganize kuti adzapulumuka ciwonongeko cimeneco . Kucokela pamenepo , anthu amene ali ndi ciyembekezo cokhala padziko lapansi kwamuyaya agwilizana ndi Akristu odzozedwa . ( Mat . 24 : 14 ) Uthenga umene timalalikila umachedwanso “ uthenga wabwino wa kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . ” Zili conco cifukwa madalitso onse amene tidzalandila mu Ufumu wa Mulungu , tidzawalandila cifukwa ca kukoma mtima kwa Yehova kumene anationetsa kupitila mwa Khiristu . ( Aef . ( 1 Yoh . 5 : 3 ) Ndipo tonse timafuna kutsatila mfundo zolungama za Mulungu mosasamala kanthu za kumene timakhala , kumene tinakulila , dziko lathu kapena mtundu wathu . Kodi mavalidwe anthu ndi mmene timadzikonzela , zimaonetsa kuti timalemekeza Yehova na anzathu , kapena ayi ? Tsopano , Katherine ndi wokondwa kutumikila monga mpainiya wapadela pacilumba ca Pacific ca Kosrae . Sindiiwala abale okhwima mwauzimu amene ndinali kutumikila nao . ( Luka 11 : 13 ) Mzimu woyela ungakuthandizeni kumvetsetsa maganizo a Mulungu . N’cifukwa cake anakhala zitsanzo zabwino za anthu a cilungamo , ndipo zinthu zinawayendela bwino mu umoyo wawo . 24 : 45 ) Tiyenela kutsatila kwambili malangizo amenewa cifukwa cakuti moyo wathu wosatha umadalila pa kumvela . — Aheb . Baibo imeneyi inafalitsidwa koyamba mu 1611 . ( Luka 6 : 13 , 14 ; Machitidwe 1 : 13 , 14 ) Conco m’malo mocititsa wacinyamata wanu kudzimva kuti palibe cinthu ciliconse cimene amacita bwino , muyamikileni ndi kumulimbikitsa . Anthu ambili adziŵa kuti kukoka fodya kumayambitsa matenda osapatsilana monga kansa , matenda a mtima , ndi kusagwila bwino nchito kwa mapapo . 28 : 19 , 20 Conco , mu July 1953 , n’nali na mwayi wopezeka pa msonkhano waukulu wakuti Anthu a m’Dziko Latsopano , umene unacitikila m’delalo . N’nali kum’tulila nkhawa zanga m’pemphelo . Tate wacikondi amaganizila mwakuya za tsogolo la ana ake . Musaiŵale kuti tifunika kupilila kuti Mulungu apitilize kutikonda . — Aroma 5 : 3 - 5 ; Yakobo 1 : 12 . Nsanja ya Mlonda iyi ifotokoza zimene Baibo imakamba pa nkhani ya moyo na imfa . Iye anatsutsa mwamphamvu cinyengo cawo mwa kukamba kuti : “ Kodi angaphunzitse bwanji [ anthu ] kumvela malamulo onse a Yesu Khiristu , ngati iwo safuna kuthandiza anthu wamba kuŵelenga Uthenga wa Mulungu m’cinenelo cawo ? ” — Aroma 10 : 14 . M’zaka 100 zoyambilila , mtumwi Paulo anacenjeza kuti : “ Mau ouzilidwa amanenadi kuti m’nthawi zam’tsogolo , ena adzagwa pa cikhulupililo , cifukwa comvetsela mau ouzilidwa omwe ndi osoceletsa , ndiponso ziphunzitso za ziŵanda . ” 2 : 16 . MTENGO wakale wa maolivi sukhala wokongola kwenikweni tikauyelekezela ndi mtengo waukulu wa mkungudza wa ku Lebanon . Mlendoyo anali Joseph F . Baibulo limati : “ Nthawi zonse mau anu azikhala acisomo , okoma ngati kuti mwawathila mcele , kuti mudziŵe mmene mungayankhile wina aliyense . ” Cinthu cosaiŵalika n’cakuti mu 1994 , zofalitsa zathu zinayamba kupulintiwa m’citundu ca Cikigizi . [ Bokosi papeji 5 ] Dziko Lathu Koma cikhulupililo cathu cingayesedwe tikaona kapena tikacitilidwa zinthu zimene tiona kuti n’zopanda cilungamo mumpingo . Kuti mudziŵe zambili za Ufumu wa Mulungu , onani nkhani 8 m’buku yakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse yofalitsidwa na Mboni za Yehova . Tsopano tiyeni tikambilane za citsanzo cangwilo ca Yehova pa nkhaniyi . 9 : 7 . Mwamuna amene amagwila nchito mwamphamvu kuti asamalile banja lake amathandiza anthu a m’banjalo m’njila ziŵili . Akulu aluso amaonanso kuti n’kofunika kuyamba kuphunzitsa abale acinyamata mwa kuwapatsa zocita mumpingo molingana ndi msinkhu wao . Zimenezi zisanacitike , Eliya anacita cozizwitsa cimene cinaonetsa kuti Yehova ndi Mulungu woona . Pambuyo pa cozizwitsa cimeneci , aneneli a Baala okwana 450 anaphedwa . ( 1 Maf . Pokhala Mfumu ya Ufumu wa Mulungu , Yesu Kristu adzacotsa ciwawa , kupondelezana , ndi kuipa padziko lapansi . Lekani n’kuuzeni cifukwa cake . Taonanso kuti atumiki akale a Mulungu anali na ciyembekezo cakuti pa nthawi ina m’tsogolo , akufa adzaukitsidwa . 15 : 21 ) Kodi tingakhale bwanji ozindikila ? ( Machitidwe 19 : 11 , 12 ; 20 : 9 , 10 ) Ngakhale kuti mapemphelo ake sanayankhidwe mmene anali kufunila , Paulo anayamikila thandizo la Yehova . — 2 Akorinto 12 : 9 , 10 . Mosakaikila , aliyense wa ife ali ndi mbali inayake m’Baibulo imene amakonda kwambili . Conco , mouzilidwa iye analembela Timoteyo kalata yomaliza . Anaphunzilanso kuti sayenela kudela nkhawa kwambili za tsiku lotsatila . ( Mat . Kodi Paulo anaonetsa bwanji kuti zocita zake zinali zogwilizana ndi malangizo ake a pa 2 Akorinto 6 : 1 ? Pambuyo pa zaka ziŵili , n’naikiwa kukhala mpainiya . Panthawiyo , n’nali na zaka 16 . Pambuyo poukitsidwa , Yesu anauza otsatila ake kuti ayenela kupanga ophunzila , ndi kuwaphunzitsa kusunga “ zinthu zonse ” zimene analamula . Koma Baibo imatiuza kusankha kuika patsogolo zinthu zauzimu , ndi kukondweletsa Mulungu m’malo modzikondweletsa tekha . Nadine anati : “ Anthu ambili amene timakumana nawo mu ulaliki , amakondwela tikamaphunzila nawo Baibo . Iye anali kukumbukila magulu a ofalitsa akulalikila kwa masiku athunthu pa manjinga , ndiyeno m’madzulo anali kuliza nkhani zojambulidwa . Iwo analamulidwa kupanga ophunzila kucokela ku “ mitundu yonse ” ya anthu . Pambuyo pake , mlongoyo anatumikila monga mpainiya kwa zaka zoposa 70 . Zocitika zimenezi zimafuna kufufuza , ndipo kufufuzako kungakhale kosangalatsa . Ngati sanadzifufuze , iye ‘ angadye ndi kumwa cilango cake . ’ Mau olembedwa a Yehova amatiunikila za gulu lake lakumwamba . Iye anangondisiya ndipo usikuwo ndinamaliza kuŵelenga bukulo . Ngakhale n’telo panali mtengo umene Yehova Mulungu anaumuuza momveka bwino kuti asadye zipatso zake . Adamu anaphunzilanso mmene angasamalile zosoŵa zake , ndi mmene angasamalile nyama na dziko lapansi . ( Aheberi 12 : 6 ) M’Baibulo , timaŵelenga za atumiki okhulupilika amene Yehova anaphunzitsa kuti akhale anthu abwino . Anafunika ‘ kupitiliza kubala zipatso zoculuka . ’ Aisiraeli anacita mantha . ( Luka 4 : 5 , 6 ) Conco , sitiyenela kupangitsa anthu ena kuganiza kuti wolamulila winawake wa boma amatsogoleledwa ndi Mdyelekezi . Koma kodi pali zinthu zina zimene Mulungu amaona kuti ni za mtengo wapatali kuposa dayamondi ndi miyala ina ya mtengo wapatali ? Njila imene Lefèvre anaseŵenzetsa inathandiza kwambili Luther kuphatikizapo womasulila Baibo dzina lake William Tyndale na katswili wina wotsutsa ziphunzitso za Katolika , dzina lake John Calvin . Masiku ano , Mkhristu akacita chimo lalikulu afunika kuonana na akulu mumpingo kuti amuthandize . N’zoona kuti maluŵawo ni ake kale tateyo . Yakobo analemba kuti : “ Mphatso iliyonse yabwino ndi yangwilo imacokela kumwamba , pakuti imatsika kucokela kwa Atate wa zounikila zonse zakuthambo , ndipo iye sasintha ngati kusuntha kwa mthunzi . ” Ena akhala ndi zotsatilapo zabwino mwa kugwilitsila nchito ulaliki wa pafoni , ulaliki wa ku dooko , kapena ulaliki wa poyela , ngakhale kuti sanadziŵe mmene njila zatsopano zimenezi zidzathandizila . Mfumu Herode inakwiya kwambili pamene openda nyenyezi anaifunsa za ‘ mfumu ya Ayuda imene inabadwa , ’ ndipo inakonza zakuti iphe khandalo . Vegetius anakamba kuti ulendo wa pamadzi unali kukhala bwino kuyambila mwezi wa May 27 mpaka September 14 . Koma masiku oyambila pa September 15 mpaka November 11 komanso March 11 mpaka May 26 anali okaikitsa . Kodi mau a Yesu amaonetsa bwanji kuti iye anali wozindikila ? Nanga zinthu zinali bwanji pamene Sisera ndi asilikali ake anali kulamulila dziko ? Muzitsanzila Mulungu Amene Watilonjeza Moyo Wosatha Ngakhale kuti Yesu anakumana ndi ziyeso zoopsa , iye anakhalabe wokhulupilika kwa Mulungu , ndipo anacilikiza ulamulilo wa Yehova . Cifukwa cakuti ali ndi cikumbumtima . N’cifukwa ciani tifunika kum’konda Mulungu ? Conco , kuti timvele kukoma kwa cakudyaci , sitiyenela kucidya mothamanga . Conco , tiyeni tizicita zimene watiuuza mokondwela cifukwa “ Mulungu amakonda munthu wopeleka mokondwela . ” Kodi anali ndi nkhawa kuti munthu wina adzamuloŵa m’malo ? Kodi tiyenela kumvela bwanji poona kuti tinamasuka ku Babulo Wamkulu ? Kodi Solomo anawononga bwanji ubwenzi wake na Yehova ? Baibo si buku wamba . 4 , 5 . ( a ) Ndi vuto lanji limene mtumiki wa m’fanizo la Yesu anakumana nalo ? Osonkhanitsidwawo tsopano ni “ mtundu wamphamvu ” wa anthu acimwemwe oposa 8 miliyoni , amene “ akucitila [ Mulungu ] utumiki wopatulika usana ndi usiku . ” ( Chiv . 7 : 9 , 15 ; Yes . N’cifukwa ciani tiyenela kupemphela kuti dzina la Mulungu liyeletsedwe ? Koma muziionanso monga nsembe yokupindulitsani inu panokha . 147 : 1 . Ndiye conde , unene kuti ndiwe mlongo wanga kuti zindiyendele bwino . Ukatelo upulumutsa moyo wanga . ” Ndipo Yesu anakambilatu kuti anthu a ciphamaso adzalandila “ cilango coopsa . ” Sitiyenela kukaikila kuti Yehova nthawi zonse amacita zinthu zoyenela ndi zacilungamo Conco , pamene tinalandila utumiki watsopanowu , n’nakhala na nkhawa . Didier na mkazi wake Nadine anacoka ku France kupita ku Madagascar mu 2010 . Kuyambila nthawi imeneyo , ine , Ilias , ndi mlongo wathu wamng’ono , dzina lake Efmorfia , tinayamba kuphunzila Baibo . Tinalinso kupezeka pa misonkhano ya Mboni nthawi zonse . Kodi mfundo za m’nkhani ino zakuthandizani bwanji ? Bungwe Lolamulila lapatsa othandizila ao amenewa nchito yaikulu , ndipo limayamikila abale okhulupilika amenewa cifukwa ca nchito imene amagwila mwakhama . ( Yoswa 23 : 1 , 2 , 14 ) Ayuda sanatsutse kuti Mulungu anakwanilitsa malonjezo ake . 1 : 2 ) Yakobo anali kukamba za mayeselo obwela cifukwa ca cizunzo ndi kupanda ungwilo kwathu . Kucita zimenezi kunam’thandiza kupilila mayeselo aakulu . N’cifukwa Ciani Tiyenela Kupemphela ? Kodi Mulungu Amakuona Bwanji Kukoka Fodya ? Ndiyeno , pa Ciŵili m’maŵa tinali kupita ku mpingo wina . M’baleyo anati : “ N’tafika pa malo olandilila alendo na kuona mmene wolandila alendo anavalila , n’nazindikila kuti ni wa mtundu umene umakamba cinenelo cimene n’naphunzila . Apolisi amangokhalila kundifunafuna . Kodi simukuvomeleza kuti Mau a Mulungu ni amphamvu mu ulaliki ? — Mac . ( Luka 10 : 40 - 42 ) Ngati munthu wokhulupilika Marita anatangwanika na zinthu zina pamene Yesu analipo , ndiye kuti na ise zaconco zingaticitikile . Kodi tingapewe bwanji msampha wokonda zinthu zakuthupi ? Nanga tingacepetse bwanji zocita zathu mu umoyo kuti tiike zinthu zauzimu patsogolo ? Inde , ndalama “ zonse zimene akanatha kucilikiza nazo moyo wake . ” Tiyeni tizidalila Yehova ndi kupemphela kwa iye ndiponso kukhala paubwenzi wolimba ndi abale ndi alongo athu a mumpingo . Pezani cilimbikitso kwa akulu acikristu ndipo yesetsani kucita zinthu zakuuzimu nthawi zonse . AMERICA : Mu 2012 , anthu 25 ku Brazil anawapeza ndi mlandu wogwilitsila nchito ndalama za boma pokopa anthu kuti akawavotele pa masankho . Kodi mfundo zimenezi tingazigwilitsile nchito motani pankhani ya ampatuko mu mpingo ? Bwanji osaganizila zolinga zauzimu zimene muona kuti n’zofunika kwa imwe , na kuyamba kuseŵenzelapo kuti muzikwanilitse ? — Ŵelengani Afilipi 1 : 10 , 11 . 115 : 10 - 12 ; 135 : 19 , 20 . Patapita nthawi , anakhala kalembela wa cipani candale cimene cinali m’mudzi wao . TENGELANI CIKHULUPILILO CAWO INOKI Ciyembekezo cathu codzakhala ndi moyo wosatha m’dziko latsopano la Mulungu , cidalila pa kukhala na cikhulupililo colimba ndi kucisunga . Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo — Mbali 1 ( Onani bokosi lakuti , “ Amayamikila . ” ) ( b ) Nanga inu panokha mwapindula motani ndi Kulambila kwa Pabanja ? Muzitsanzila Yehova mwa kusonyeza cikondi ( Onani ndime 7 ) Ndipo abale ambili akakhala paudindo , aliyense mumpingo amapindula . Iye anali kutsidya lina la Nyanja ya Ejani , m’cigawo ca Asia Minor . ( Yohane 3 : 16 ) Ngakhale kuti zimenezi zinali zopweteka kwambili kwa Yehova , iye analola kuti Mwana wake aphedwe monga dipo . Koma zambili zimene munthu wolemela amakhala nazo zimamulepheletsa kugona . ” — Mlaliki 5 : 12 . Ndinali kumvetsela mwachelu ndi kuona zimene zinali kucitika . Mfumu yakale Solomo anali na cidziŵitso coculuka ponena za njila za Yehova . Conco , potumikila Yehova mumpingo wa cinenelo cina , tingacite bwino kuteteza umoyo wathu wauzimu . — Mat . Ngakhale kuti tinali kugwilabe nchito yomasulila Cituvalu , tinali kuthandizilanso anthu omasulila Cisamowa , Citongani , ndi Citokelauni . Ndiyeno , Yesu anachula mfundo ya coonadi yofunika kwambili imene ngakhale otsatila ake masiku ano amaitsatila . Iye anati : “ Onse ogwila lupanga adzafa ndi lupanga . ” — Mat . Ndingakonde kudzakumananso nanu pano kuti ndidzamve maganizo anu pa kamutu kakuti “ Kodi Mungacite Ciani Kuti Cikwati Canu Cipitilize ? ” Anali kupita naye “ kudziko la Sinara , ” kapena kuti ku Babulo . Pamene mtumwi Petulo anafunsa kuti ndi nthawi zingati pamene angakhululukile mnzake , Yesu anam’yankha kuti : “ Mpaka nthawi 77 . ” ( Mat . A Inoki : Panthawi ina , anthu anali kutsutsa kuti munthu wochedwa Mfumu Davide analiko . Ndipo Baibo imati : “ Mawu a Mulungu ndi amoyo ndi amphamvu . ” Popeza timakhala na zocita zambili , timafunika nthawi yopumulako ndi kucitako zosangulutsa . ( a ) Ni mafunso ati amene tiyenela kudzifunsa ? Ni anthu ati amene sakhala na cimwemwe ceni - ceni ? Cifukwa iye ndi amene angakwanilitse zofuna zao ndipo amakwanilitsa zimenezo kudzela m’Mau ake Baibulo . Mtengo umenewu unali wolingana ndi malipilo amene munthu wamba anali kulandila akagwila nchito kwa masiku 25 . Kodi ndimadandaula za amene akutsogolela mumpingo ? Malinga ngati dziko la Satana lilipo , sitingatumikile Yehova mmene tingafunile . Hava “ anayamba kuona kuti zipatso za mtengowo n’zokoma kudya , zokhumbilika ndi zosililika . ” Mu September 1919 , Ophunzila Baibulo anacita msonkhano wa masiku 8 ku Cedar Point , Ohio , m’dziko la U.S.A . Cifukwa ca mphamvu zazikulu za Yehova , ‘ dzuŵa linaima , ndiponso mwezi unaima mpaka mtunduwo utalanga adani ake . ’ ( Yeremiya 25 : 10 ) Mphelo zazikulu zoyendetsedwa ndi nyama zinali kugwilitsilidwa nchito ndi anthu ogaya ufa osati akazi apanyumba . — Mateyu 18 : 6 . Koma ofalitsa ena anali olimba mtima kwambili . Iwo anali kukwanitsa kuuza mwininyumba zinthu zambili pa nthawi yocepa . Tinakhala mu mzinda wa Mistelbach kwa caka na miyezi . 4 , 5 . ( a ) Kuwonjezela pa kulalikila , kodi tingaonetse bwanji kuwala kwathu ? Ndiponso , Yehova analamula kuti ngati munthu wapha nyama kuti akadye , anayenela kuthila magazi ake pansi ndi kuwafotsela . Kumeneko , iye anapatsa Sauli ndi mtumiki wake malo apamwamba kwambili ndi nyama yabwino . Ndiyeno Samueli anati : “ Tenga , udye cifukwa anasungila iweyo kuti udzaidye panthawi ino . ” Pa nthawi ya nkhondo yoyamba ya dziko lonse , kodi cinali kucitika n’ciani pakati pa Ophunzila Baibo na Babulo Wamkulu ? Yesu anakamba kuti “ pakamwa pamalankhula zosefukila mumtima . ” Anali kugwila nchito imeneyi modzipeleka kwambili ndiponso molimba mtima . Buku ina inati : “ Alembi aciyuda amene anakhalako m’zaka zoyambilila za Cikhristu anakopa Baibo ya Ciheberi mobweleza - bweleza , ndipo anaikopa molondola kwambili . ” — Second Thoughts on the Dead Sea Scrolls . Komabe , Danieli anali akali moyo . Ngakhale pamene anali ndi zaka 12 , iye anagwilitsila nchito Malemba pokambilana ndi aphunzitsi m’kacisi . ( b ) N’ciani cimene cingatithandize kulimbana ndi zinthu ‘ zovuta ’ ? Kokhazikika Ndithudi , ndise oyamikila ngako kuti tili na Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika limene lili na mau osavuta kumva . Koma Yehova anafunabe kuti mukhale bwenzi lake . Sindidzaopa . ” ’ ” Anasiya zinthu zonse zimene anali nazo mumzinda wa Lusitara . 3 : 10 ) Ndithudi , zinthu zonse n’zotheka kwa Yehova ! Mofananamo , masiku ano njila imodzi imene Akristu amaonetsela kuti ndi “ odzipeleka kwa Mulungu ” ndi mwa kusamalila acibale ao osoŵa mwakuthupi . Yehova ni dzina la Mulungu lopezeka m’Baibulo . ( 2 Ates . 1 : 3 - 5 ) Yehova na Mwana wake amalimbikitsa Akhristu onse okhulupilika amenewa . — Ŵelengani 2 Atesalonika 2 : 16 , 17 . Mulungu walonjeza kuti : “ Sindidzakusiyani kapena kukutayani ngakhale pang’ono . ” — Aheberi 13 : 5 Lemba lathu la caka ca 2015 lidzatikumbutsa za mfundo imeneyi kwa caka conse . ( b ) N’cifukwa ciani tiyenela kuvomeleza kufooka kwathu ngati mmene Yehosafati anacitila ? Iye anaona monga n’nanyalanyaza kupanga makonzedwe a thilansipoti ya a mishonale amene anali kubwela . Koma si mmene zinalili . Yehova adziŵa mavuto amene tikukumana nao , monga mmene anacitila ndi Aisraeli pamene anali kuvutika mu ukapolo ku Iguputo . Baibulo limayankha kuti : “ Dziko linagwedezeka , kumwamba kunagwetsa madzi . ” Ndinabatizidwa mu 1989 , ndili ndi zaka 61 . Alonda anali kuimilila pamwamba pa zipupa . Ali pamenepo , anali kukwanitsa kuona malo onse ozungulila mzindawo . Alonda ena anali kuimilila pa geti ya mzinda usana ndi usiku . Wacicepele , Limbitsa Cikhulupililo Cako , Sept . Mwacitsanzo , m’busa wina anati : “ Ine sindine wa Mboni , koma naona kuti mumagwila nchito yolalikila mwadongosolo , ndipo mumagwilizana olo kuti ndinu osiyana mitundu . ” Mwina munali kudzikambila mumtima kuti : ‘ Usakhulupilile ! Muzikonda zacilengedwe ndi kuŵelenga mabuku athu ofotokoza za cilengedwe . ( Mat . Koma khalidwe limeneli linali kum’vutitsa maganizo . Mlaliki 12 : 1 97 : 10 . Analinso kuphunzila Baibo payekha mwakhama . KUNGOCOKELA pamene anthu anacimwa na kukhala opanda ungwilo , Yehova waonetsa kuti ni Mulungu amene amapeleka cilimbikitso . Kodi n’zotheka munthu waciwawa kusintha n’kukhala wofatsa ? Nafenso tiyenela kutelo . — Aroma 15 : 15 , 16 . Anthu ambili amakhulupilila kuti pemphelo sicinthu congocita mwamwambo cabe , koma Mulungu amamvetsela mapemphelo ndipo amayankha . Ine ndi Angie tinayesetsa kukhala na umoyo wosalila zambili kuti tikhale okonzeka kukatumikila kulikonse kumene tingafunike . Ndipo nthawi zambili anthu otsatsa malonda amaseŵenzetsa anthu ooneka bwino pofuna kutisonkhezela kugula zinthu zimene n’zosafunika kweni - kweni mu umoyo wathu . Tingakonzekele bwanji cizunzo ? Nanga tingagonjetse bwanji maganizo olefula ? Mfumu Davide anayelekezela mapemphelo ake ngati zofukiza pamene anaimba kuti : “ Pemphelo langa likhale lokonzedwa ngati zofukiza pamaso panu [ Yehova ] , mapembedzelo anga akhale ngati nsembe yambeu yamadzulo . ” ( Sal . 141 : 2 ; Eks . Pokhala Mboni zake , nafenso tifunika kukhala oyela . ( Gen . 9 : 3 - 6 ) Yehova analetsa kudya magazi monga cakudya . N’nazindikila kuti cinali cikhalidwe cawo ku Philippines , kuti nkhani ya anthu onse izikambidwadi poyela . N’cifukwa ciani sitiyenela kukhalila kupeza anzathu zifukwa ? M’bale Marais woyang’anila nchito yomasulila , anafotokoza kuti abale anali kukonza zoti pakhale kosi yophunzitsa Cizungu omasulila onse padziko lonse . N’nali na zaka 64 , koma ananipempha kuti nikhale mmodzi wa aphunzitsi a kosi imeneyo . LANA sadzaiŵala zimene zinacitika tsiku lina mu 2012 ku Germany . Kodi nchito yolalikila imagwilizana bwanji ndi kukonda anzathu ? Kumam’cititsa kuzidziŵa bwino ndi kudziŵa mmene apitila patsogolo . Iye anali kum’konda kwambili mwana wake wam’ng’ono , koma apa sakanakwanitsa kukamba naye tsiku lililonse . Tsanzilani Cikhulupililo Cao | Timoteyo Munthu amene ali ndi khalidwe loyela , amapewa zinthu zoipa . Maureen , wa zaka za m’ma 60 , anakamba kuti : “ Pamene n’nali kukula , n’nali kulakalaka kukhala na umoyo wa colinga , umoyo wothandiza ena . ” Zimene zinacitikila Mose ni cenjezo lamphamvu kwa ise pa nkhani imeneyi . 6 : 10 ) Ndiponso , tiziyesetsa ‘ kuvula umunthu wakale pamodzi ndi nchito zake , ’ zimene zingatifooketse mwauzimu . — Akol . Iye anati : “ Sananipatse mwayi uliwonse wa utumiki kupatulapo kucita upainiya wanthawi zonse . ” Ngakhale zili conco , onse amazindikila kuti ali ndi udindo wokhulupilila Kristu ndi kuonetsa cikhulupililo cimeneco mwa kugwila nchito yolalikila . — Yak . ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) N’ciani cinacitika mai wina atayankha mnzake mokoma mtima ? Cisautso cacikulu cili pafupi kwambili . Conco , tifunika kukhala “ mtundu wa anthu okhala ndi cikhulupililo cosunga moyo . ” Hannah anakambanso kuti : “ Ndidziŵa kuti Yehova akanakoka mai ameneyu mwa njila ina yake . Komabe , kutumikila ku malo osoŵa kunathandiza kuti tipeze munthu ameneyu amene ali ngati nkhosa ndi kum’thandiza kudziŵa Yehova . N’ciani cimene tiyenela kucita kuti tikhalebe oyela ? Popeza nthawi zina ana amatopa , zingakhale bwino kuti tate aone kuti ndi nkhani ziti zimene angasankhe ndipo ayenela kupeza nthawi yokonzekela . Kodi mungasonyeze acinyamata mmene angalimbikitsile abale ndi alongo acikulile mwakuuzimu ? ( b ) Kodi zimenezi zinakwanilitsidwa bwanji ? Masomphenya a namba 8 komanso otsilizila a Zekariya ni olimbitsa cikhulupililo ngako . ( Miy . 24 : 29 ) Yesu anafotokoza njila yabwino yothetsela mikangano . Mlongo wina dzina lake Joyce Ellis anati : “ Abale ambili anazindikila kuti afunika kuyamba upainiya . Ngati mufuna kudziŵa zambili , mungafunse ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova ya m’dziko lanu . Ngati mumakhala ku malo osungila okalamba , bwanji osapanga malowo kukhala “ gawo ” lanu mwa kulalikila kwa ogwila nchito ku malowo ndi anthu ena okhala kumeneko ? Zikuoneka kuti anthu ambili m’gulu limenelo anakhala Akristu . 24 : 45 ) Abale a m’bungweli amapemphela kuti apange zosankha zoyenela . Davide asanafe , Yehova anam’lonjeza kuti ufumu wake udzakhala kosatha . Mulungu anati : “ Ndidzautsa mbeu yako yobwela pambuyo pako , imene idzatuluka m’ciuno mwako . Ndipo ndidzakhazikitsadi ufumu wake . ” ( 2 Sam . ( Ŵelengani Aheberi 12 : 1 . ) Cifukwa ca citsanzo cao , ndaphunzila kuti ndiyenela kugwila nchito mwamphamvu kuti ndicite zinthu zimene zingathandize ena . ” Caciŵili , pofuna kumuonetsa cifukwa cake amamudela nkhawa , Don anauza Peter kuti aŵelenge pa Aroma 10 : 13 , 14 , pamene pamakamba kuti “ aliyense amene adzaitana pa dzina la Yehova adzapulumuka . ” ( Yelekezelani na 2 Mbiri 13 : 7 . ) Ndi zolinga ziti zimene alengezi a Ufumu angakhale nazo ? M’nkhani yapita , tinaphunzila kuti m’zaka zaposacedwapa , kapolo wokhulupilika wasintha mofotokozela nkhani zina za m’Baibulo . Masiku ano , kapolo wokhulupilika akufotokoza kwambili zimene tikuphunzilapo pa nkhanizo m’malo molongosolo zimene ulosiwo kapena nkhaniyo ikutanthauza . Tsiku lina pokambilana za m’Baibo , tinayelekeza mmene dziko lilili masiku ano na maulosi ali pa Mateyu caputa 24 , Luka caputa 21 na pa 2 Timoteyo caputa 3 . Iye anali ndi mphamvu yocita zimenezo . ( 1 Akor . 15 : 58 ) Nchito zimenezi zingaphatikizepo nchito yomanga , kukonzanso maholo kapena mabwalo olambilila , nchito zokhudza misonkhano ya dela ndi ya cigawo , kapena kutumikila pa ofesi ya nthambi kapena pa ofesi yomasulila mabuku . Ambili a io amagwila nchito maola 130 pa mwezi mu ulaliki . Conco , atumwi anasankha amuna oyenelela kuti asamalile akazi amasiye ndi kuwagaŵila cakudya cokwanila . ( Mac . Atumiki anthawi zonse amakalamba , cimodzimodzinso makolo ao . Patapita caka cimodzi ndi hafu Yesu atakumana ndi Natanayeli ( amenenso anali kuchedwa kuti Batolomeyo ) , anamupatsa udindo wofunika kwambili . ( 2 Samueli 12 : 9 - 12 ) Koma Yehova anamucitila cifundo ndi kumukhululukila . Yehova angatithandize kupilila mavuto amene angaoneke monga osapililika malinga ngati tikhalabe okhulupilika kwa iye Mu 2008 anasamukila ku Russia . M’bale Mumba : Muli bwanji a Daka ? Polembela Akhiristu ku Roma , Paulo anati : “ Ndikuuza aliyense wa inu kumeneko kuti musamadziganizile kuposa mmene muyenela kudziganizila . Mu 313 C.E . , Mfumu ya Roma yacikunja dzina lake Constantine , inavomeleza mwalamulo Cikhiristu ca mpatuko kukhala Chechi yovomelezeka . Mwacionekele , mgwilizano umenewo unacititsa kuti azikondana kwambili . Zimenezo zingam’thandize kuti amasuke kukamba mmene tsiku lake layendela . Tili pa nyumba ya wailesi ya WBBR pamodzi na M’bale Franz Akristu amenewa ndi citsanzo cabwino kwambili kwa ife cifukwa anasonyeza zimene zingatithandize kupilila . Ngati n’conco , ni liti ? Nanga n’cifukwa ciani amacita zimenezi ? Iye anali kuwadziŵa bwino Malemba cifukwa cakuti amai ake ndi ambuye ake aakazi anam’phunzitsa Malemba . Ndisanafotokoze cimene camucititsa kuona moyo kukhala wofunika , ndiloleni ndikuuzeni mbili yake . Komabe , nthawi zina io amakhala ndi nchito zina zoonjezeleka . Kodi n’zotheka kupambana polimbana ndi Satana ? Khalani patsogolo poonetsa ulemu kwa ena . Conco , palibe cifukwa ca m’Malemba cofuna kudziŵila ngati cocitikaci cili ndi tanthauzo lobisika . — Gen . ( b ) Pokhala Akristu , tili ndi udindo wotani ? Kuti anthu amene ali m’comboco apulumuke , afunika kusambila mpaka kumtunda . M’nthawi ya mapeto , makamaka kuyambila mu 1919 , akapolo odzozedwa a Kristu ndiponso okhulupilika padziko lapansi , akhala akucita malonda ndi matalente a Mbuye wao . Monga mmene analili ndi mphamvu zoukitsa Lazaro , Yesu alinso ndi mphamvu zoukitsa anthu mtsogolo . Mulungu anakokela kwa iye ndi kwa Mwana wake anthu ambili amene anali kuonedwa otsika . Conco inuyo . . . musankhe moyo kuti mukhalebe ndi moyo . ” — Deuteronomo 30 : 19 Mneneliyo anatuma mtumiki wake Gehazi kuti atsogole kupita ku Sunemu . Kumbukilani kuti tsiku lina , tidzacita Cikumbutso cothela . “ Popeza imfa inafika kudzela mwa munthu mmodzi , kuuka kwa akufa kunafikanso kudzela mwa munthu mmodzi [ Yesu ] . ” — 1 Akorinto 15 : 21 . Pamene n’nali kutumikila kumeneko , n’nayamba kuganizila za Nora , amene n’nayambila naye limodzi kucita upainiya . Pamene anali padenga la nyumba yake , iye “ anaona mkazi akusamba . ” PALI nthano ina yakale , imene imakamba za kamnyamata kosauka kamene kanali kukhala m’mudzi wakutali . Conco , thandizo limene acibale ndi mpingo ungapeleke kwa abale ndi alongo okalamba limasiyana - siyana . Anawauza kuti sanabwele kudzawapatsa zinthu zakuthupi , koma kudzawaphunzitsa za Ufumu wa Mulungu . Pa msonkhano wacigawo mu 2006 , panakambiwa nkhani imene inam’fika pamtima Daniel . M’nkhaniyo , munali funso lakuti : “ Kodi tikuchita zomwe tingathe pothandiza omwe ‘ akuyenda movutikira popita kukaphedwa ’ kuti abwere pa njira ya kumoyo wosatha ? ” ( Miy . Muzipewa kuyelekezela mpingo wanu watsopano na wakale . ( 1 Akorinto 9 : 5 ; 1 Petulo 3 : 5 , 6 ) Kukamba zoona , sembe Sara anakhala zii osakambapo ciliconse , zikanaonetsa kuti sakulemekeza Abulahamu , cifukwa zinthu sizikanayenda bwino kwa mwamuna wake komanso m’banja lawo lonse . Kodi anthu amene amacilikiza ulamulilo wa Mulungu amapanga bwanji zosankha ? Abale a ku Filipi ayenela kuti anali kulimbikitsidwa ngako akaganizila zimene zinacitika mu zaka 10 kucokela pa nthawi imene Paulo na Sila anapulumutsidwa ndi Mulungu mozizwitsa . Mwacitsanzo , ngati muli pa cibwenzi muyenela kukumbukila kuti cilakolako cakugonana ndi camphamvu kwambili . Mame amapangika pang’onopang’ono pamene mpweya umasintha ndi kupanga tumadontho twa madzi . Ganizilani zimene iye anacita kwa Yesu . Mu 500 B.C.E . , Nehemiya anada nkhawa atadziŵa kuti ana ena pakati pa Ayuda amene anabwelela ku Babulo , anali kukangiwa kukamba Ciheberi . Njilayo ‘ Anali Kuidziŵa ’ ( G . Komabe , mbadwa zambili za Adamu zasankha Yehova kukhala Wolamulila wawo . Mofanana ndi wamasalimo , ‘ nyimbo yathu imanena za mfumu ’ imene ndi Yesu Kristu . Ngati tipemphela m’njila yovomelezeka ndipo timapempha zinthu zoyenela , Mulungu adzatimvetsela . Makolo ndi ana akamapatula nthawi yophunzila za Yehova pamodzi , amayamba kukondana kwambili . Pamene tikambilana za ufulu , ni bwino kukumbukila kuti Yehova Mulungu yekha ndiye ali na ufulu wocita ciliconse — ufulu wopanda malile . Panthawiyo , ine na amayi tinali kukhala m’tauni yaikulu ya Karachi . Paciyambi , dziko lapansi linali “ lopanda maonekedwe enieni ndiponso lopanda kanthu . . . Ndipo pamwamba pake panali mdima wokhawokha . ” Cilamulo ca Mose cinafotokoza zinthu zimene zingadetse munthu . Ngati timaona kuti zinthu zimenezi ndizo zofunika , ndiye kuti tikusoŵa cinthu cina cofunika kwambili cimene ndi cuma cakuuzimu . Ngati tayamba kuona kuti Yehova satikonda , tiyenela kukumbukila kuti ndife a mtengo wapatali kwa Yehova , ndiponso kuti iye ‘ wagwila dzanja lathu lamanja ’ kuti atithandize . Koma Mose anamuyankha kuti : “ Kodi ukucita nsanje cifukwa condidela nkhawa ? Kodi wacita zimenezi cifukwa colema kapena cosamva bwino ? Iye anadziŵa kuti citsanzo cake cabwino cidzathandiza ophunzila ake . Pamene tinayamba kuphunzila Baibo , mwina abululu athu sitinawauze kuti tayamba kugwilizana ndi Mboni za Yehova . Lonjezo la kudzipeleka ( Onani palagilafu 10 ) Monga aphunzitsi m’banja , mpake kuti makolo amafuna kuti ana awo akhale na cidziŵitso cokwanila cimene cingasonkhezele anawo kudzipeleka . CAKA COBADWA : 1958 15 : 7 , 11 ; Lev . Kwa nthawi ndithu , n’nafunika kukhala osaseŵenza kuti mphamvu zibwelelemo , koma n’tacila , tinayambanso utumiki wa nthawi zonse . Komabe , iye amatitsimikizila kuti : “ Ndidzakupatsa malangizo ndi kukuyang’anila . ” — Salimo 32 : 8 . Tifunika kumapezeka pa misonkhano yampingo nthawi zonse . ( Yes . 32 : 1 , 2 ) Kukamba zoona , makonzedwe amenewa amaonetsa cifundo ca Mulungu . Palinso cifukwa cina cimene ciyenela kuti cinacititsa Yehova kukwiyila Mose na Aroni . Ngakhale kuti Yehova ali na zonse , n’ciani cimene ife tingamupatse ? Ofalitsa Ufumu ku Japan anayamba kugaŵila bukuli mokangalika kunyumba ndi nyumba ndi pa maulendo obwelelako . ( b ) Nanga iwo anayankha bwanji Mulungu atawalamula kuti ayenela kukhala okhulupilika kwa iye yekha ? 18 : 10 . Mkulu wina dzina lake Frédéric , amene anapempha wacicepeleyu kuti aziphunzila naye , anati : “ Ndinamuyamikila Rico cifukwa zimene anacita pamene anakumana ndi citsutso cimeneco , zinaonetsa kuti sanacite mantha kukamba za cikhulupililo cake . ” Kamvedwe katsopano : Yesu sanali kulosela kuti otsatila ake ena odzozedwa adzakhala oipa ndi aulesi . Tingadziikile zolinga monga kunola luso lathu m’mbali zina za utumiki . Mwacitsanzo , ataopsezedwa na Esau , Yakobo anapempha Mulungu kuti : “ Ndapota nanu [ conde ] , ndipulumutseni . . . Monga mmene kusintha kwa mwadzidzidzi kwa pa nyanja kunacenjezela anthu okhala ku Simeulue za kubwela kwa tsunami , zocitika za padzikoli zikuticenjeza kuti mapeto ali pafupi . Ngakhale kuti kusamalila maudindo ambili ndi nchito yovuta kwambili , Michael amene akutumikila monga mkulu tsopano akupitiliza kunena kuti : “ Kuthandiza abale kwandicititsa kukhala wokhutila . ( Sal . 102 , tumau twa pamwamba ) Mau ake amaonetsa kuti iye anakhudzidwa kwambili ndi mavuto ake , ndipo anasungulumwa . ( Sal . Ndi mfundo ziŵili ziti zimene tikuphunzila m’fanizo la matalente ? Mu 1492 , Christopher Columbus , katswili wofufuza malo waciitaliyani , anaona kuti watsala pang’ono kupeza munda wa Edeni atafika pa cisumbu ca Hispaniola , cimene tsopano ni maiko a Dominican Republic ndi Haiti . Ndipo khalani wodzicepetsa m’malo mongofuna cabe udindo . — Mat . ( Salimo 46 : 9 ) Koma anthu okonda mtendele , “ adzasangalala ndi mtendele woculuka . ” — Salimo 37 : 11 . Ataganizila malo angapo kumene angapite , analemba kalata ku ofesi ya nthambi ya ku Guam , ndipo anam’thandizila kumene angapita . Mlongoyu anali wa ku Hungary ndipo analandila adilesi ya munthu amene amalankhula Cihangariya kuti aziphunzila naye . ( Chiv . 18 : 2 , 4 ) Mu 1919 pambuyo pankhondo , panayambika nchito yapadziko lonse yolengeza za njila ya Mulungu yopulumutsila anthu ndi za Ufumu umene unakhazikitsidwawo . Kodi lemba la Mateyu 24 : 37 - 39 limaonetsa ciani ponena za mmene zinthu padzikoli zidzakhalila m’masiku otsiliza ? M’fanizo la wofesa mbeu , Yesu anakamba kuti ena adzavomeleza “ mau a ufumu , ” ndipo adzapita patsogolo kwakanthawi , koma ‘ nkhawa za m’nthawi ino ndi cinyengo camphamvu ca cuma cidzalepheletsa mauwo kukula . ’ ( Mat . Cinanso , tiphunzilapo kuti olambila ake okhulupilika afunika kudana kwambili na zoipa . Christine , mpainiya wa ku Germany amene ali ndi zaka za m’ma 30 anati : “ Zoona , kutumikila ku malo osoŵa n’kosangalatsa . ” Koma anachulanso zifukwa zina zotamandila Mulungu . Satana , amene ni katswili wofalitsa mabodza , amadziŵa zimenezi . Tidzapeza madalitso anji cifukwa ca dipo ? Mtumwi Yohane analimbikitsa Gayo ndi kum’tsimikizila kuti anali kucita zinthu zabwino . Patrick , m’bale wa ku Africa , anati : “ Maganizo anga ali monga bokosi la mameseji lodzala ndi zinthu zambili , zoyenela ndi zosayenela . 13 Khalani ndi Cikhulupililo Ndipo Muzipanga Zosankha Mwanzelu Ricardo , amene anatsitsidwapo pambuyo potumikila monga mkulu kwa zaka zambili , anati : “ Ndinakhumudwa kwambili cifukwa ndinaona monga ndalephela . Potsilizila , mu January 1965 , tinakambilana ndi ofesi ya nthambi . ( Luka 22 : 19 ) Mboni za Yehova zidzakumbukila imfa ya Yesu pa Ciŵili , April 11 , 2017 , dzuŵa litaloŵa . ( b ) Kodi Kristu adzagwilitsila nchito motani lupanga lake mtsogolo ? Iwo anapempha anthu amene anakondwelawo kuti asawalambile . Coyamba , Ababulo anaononga Yerusalemu mu 607 B.C.E . , kenako asilikali a Aroma anaononga mzindawo mu 70 C.E . Tifunika kukumbukila kuti pa nthawi inayake , ise tonse tinali “ alendo , ” otalikilana ndi Mulungu . ( Aef . Kodi angelo akanakamba kuti anali ‘ osayenelela ’ monga mmene Yakobo anakambila ? Kapena kodi akanazimva ‘ ocimwa ’ monga mmene Petulo anamvelela ? ( Gen . Kuganizila zimene mwana wanu angacite , zimene sangacite , ndi zinthu zina kudzakuthandizani kulanga bwino ana anu ndiponso moyenela . KULANGA MOSASINTHASINTHA Cifukwa caciŵili n’cakuti kuciyambi kwa zaka za m’ma 1500 , amuna ena analimba mtima ndi kumasulila Mau a Mulungu m’zinenelo zimene anthu analukamba . Kuyambila nthawi imene Satana anapanduka , ziŵanda ndi anthu akhala akutsutsa mfundo ya coonadi yofunika imeneyi . Yosimbiwa na Thomas Mclain Yehova ataona kuti Kaini watsala pang’ono kucita coipa , anayesa kum’thandiza mwa kum’funsa kuti : “ N’cifukwa ciani wapsa mtima conco , ndipo nkhope yako yagwelanji ? Onse aŵili Adamu ndi Hava anacimwa , koma Adamu ndiye anaimbidwa mlandu pa ucimo wao . Sitingapewe matenda ndi imfa . Ndipo sitingakhalenso paubale ndi Mulungu mwa ife tekha , ndi kukhala wopanda mlandu kwa iye . Luis ndi Dale Ndinali kudzifunsa kuti , ndidzasunga bwanji ana anga aŵili ? ” — Janet , wa ku United States . M’madela ena , cimaoneka cacilendo anthu a mitundu yosiyana - siyana kusonkhana pamodzi kuti alambile Mulungu . Ndipo anthu ena amaipidwa nazo . PANTHAWIYI , Yudeya anali kulamulidwa ndi Aroma , moimilidwa ndi bwanamkubwa pamodzi na gulu lake la asilikali . Kudziŵa izi , kumatisonkhezela kuphunzitsa ena mwakhama coonadi ponena za Mulungu wathu . ( 1 Timoteyo 2 : 4 ) Timaonetsa kuti timakonda Yehova ndi anthu mwa kulalikila mwakhama za Ufumu wa Mulungu ndi zimene udzacitila anthu . — Ŵelengani Salimo 66 : 16 , 17 . Anthu aconco sakhala na cimwemwe ceni - ceni . N’nawayankha kuti : “ Ngati n’kotheka , olo lelo tingayambe ” Amakhala okhutila na zimene ali nazo Cotelo , simufunika kucita kupita ku tuakacisi kukapemphela poganiza kuti m’pamene Mulungu adzayankha mapemphelo anu . Kugwilizana ndi anthu oipa kungakucititseni kusamvela Yehova , koma kugwilizana ndi anthu abwino kungakuthandizeni kukhala okhulupilika kwa iye . Kwa maola ambili tinayankha mafunso ao ndi kuimba nao nyimbo za Ufumu ndipo tinadyela limodzi cakudya ca madzulo . ( 1 Pet . 1 : 15 , 16 ) Cikondi ceni - ceni “ sicicita zosayenela , sicisamala zofuna zake zokha . ” — 1 Akor . Ndiye cifukwa cake , Mfumu yanzelu Solomo inati : “ Palibe munthu wolungama padziko lapansi amene amacita zabwino zokhazokha osacimwa . ” 2 : 1 - 4 . Mu 1978 , kwa nthawi yoyamba tinayenda ulendo wa pa nyanja kupita ku mzinda wa Port Moresby , m’dziko la Papua New Guinea kukacita msonkhano wa maiko . Tsiku lotsatila , n’nakumana ndi mtsogoleli wa gulu limenelo ali yekha . Komanso ena amati kumwamba kumakhala milungu yambili - mbili . Kodi mukufuna kudzakhala osangalala ? Iye ananifotokozela kuti mmodzi wa abale oseŵenzela mu ofesi yake adzaloŵa Sukulu ya Utumiki wa Ufumu , imene idzatenga mwezi wathunthu . Anafotokozanso kuti pambuyo pake m’baleyo adzayamba kutumikila m’Dipatimenti ya Utumiki . Coyamba , malinga n’zimene Mau a Mulungu amakamba , Yehova ndiye anapanga makonzedwe akuti akulu azisamalila nkhani zokhudza macimo aakulu . Kukanawathandiza kuti akhale ogwilizana ngako . Kodi munadzifunsapo kuti colinga ca moyo ndi kusangalala , kugwila nchito , kukwatila kapena kukwatiwa , kulela ana ndi kukalamba basi ? Mfundo za m’Baibulo n’zothandiza masiku ano monga mmene zinalili zaka zambilimbili zapitazo pamene linalembedwa ( Aroma 16 : 6 ) Kodi tingathandize bwanji acatsopano kudziŵa kuti kuthandiza abale ndi alongo mumpingo n’kofunika kwambili ? N’ciani cimene ena acita cifukwa cokonda Mulungu ? 10 : 16 ; Miy . 22 : 3 ) Muziwamvetsela moleza mtima akamafotokoza mavuto awo , koma muzipewa kukambilana nawo nkhani zandale . ( Yes . 25 : 8 ) Mofanana ndi tate amene akuyesetsa kuthetsa mavuto a ana ake , Yehova ndi wofunitsitsa kuononga imfa ya Adamu . Palibe amene angatilande ubwenzi wathu ndi Mulungu pokhapo ngati talola kuti zimenezi ziticitikile . Mwina ndinu wokhumudwa cifukwa ca kutha kwa cikwati canu . ( Gen . 18 : 22 - 33 ; 19 : 18 - 21 ) Komanso , kwa zaka zoposa 1,500 , Yehova anacita zinthu moleza mtima ndi mtundu wosamvela wa Isiraeli . — Ezek . M’Baibo timapezamo mau a Yesu okhazika mtima pansi . Koma Yosefe anakana ndipo anathawa . Panthawi imeneyo , cinsalu copinda cimene cinali ku pulatifomu cinatambasuliwa , ndipo panali mau akuti : “ Lengezani Mfumu ndi ufumu wake . ” Komabe , ni bwino kuzindikila kuti malo athu m’makonzedwe a Mulungu si acikhalile . Ganizilani ndemanga zocokela pansi pamtima za abale atatu amene ali ndi ciyembekezo ca padziko lapansi , ndipo atumikila kwa zaka zambili ndi a m’Bungwe Lolamulila . Ngati titumikila Yehova mokwanila , tidzakhala okhutila , acimwemwe , komanso tidzakhala ndi mtendele wa m’maganizo . Atsogoleli amenewo anali osiyana ngako ndi anthu “ okwela abulu ofiilila , ” amene anakana kukamenya nkhondo cifukwa conyada . N’ciani cimene Yezebeli anacita kuti Naboti aphedwe ? Apa , ni mpainiya wanthawi zonse ndipo aganizilanso zobwelela ku kagulu ka cinenelo cina . ” Mundawo unali pafupi ndi malo pamene Mfumu Solomo ndi asilikali ake anali kukhala . Mfumu Solomo anaona mtsikanayo ndipo analamula akapolo ake kumubweletsa kwa iye . Izi n’zimene zinacitikila bwenzi la Yesu , Marita . ( Aroma 12 : 13 ; 1 Pet . 4 : 9 ) Popeza Akhristu amaceleza abale na alongo amene abwela kudzaceza , ndiye kuti afunikanso kuceleza Akhritsu anzawo amene miyoyo yawo ili paciopsezo , kapena amene akuzunzidwa cifukwa ca cikhulupililo cawo . — Ŵelengani Miyambo 3 : 27 . Anayamba na mau akuti : “ Ine Yakobo , kapolo wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Khristu , ndikupeleka moni kwa mafuko 12 amene ali obalalika . ” Musanayankhe funsoli , ganizilani zitsanzo izi : Kwa zaka zambili , Akristu ena anali kulimbikitsa mlongo wina dzina lake Taylene kuti asamadzikaikile koma kuti azicita zimene angakwanitse . Ife sitiyenela kukhala conco . M’bale wina amene watumikila monga wothandizila kuyambila mu 1992 anati : “ Kucita mwakhama utumiki uliwonse umene ndapatsidwa , kumathandiza kuti Bungwe Lolamulila liziika kwambili maganizo ao pa zinthu za kuuzimu . ” ( Yohane 14 : 15 ) Ngati titsatila malamulo a Yesu , tidzadya mkate umenewu kwamuyaya . — Deuteronomo 12 : 7 . Ngakhale kuti combo cinamswekelapo kangapo Paulo , ndipo anakumana ndi zoopsa panyanja , Malemba sakamba mwacindunji kuti pa maulendo akewo anakumanapo ndi acifwamba . — 2 Akor . Iye anati : “ N’nali kuona kuti mtundu wanga ni wabwino kwambili kuposa ina yonse , komanso n’nangena m’cipani candale . Ngati Yesu anali kukamba za ciukililo ca kumwamba , ndiye kuti mau ake safotokoza kaya ngati anthu amene adzaukitsidwa padziko lapansi adzayamba kukwatila kapena kukwatiwa m’dziko latsopano . N’kofunika kusinthasintha makambilano athu kuti zikhale zosavuta kwa anthu kumvetsela uthenga wathu . Conco , ena afunsapo ngati n’zotheka kupempha abale ndi alongo kuleka kugwilitsila nchito pelefyumu ndi mafuta ena onunkhila akamabwela ku misonkhano yampingo , yadela , ndi yacigawo . M’buku lake lakuti Healing a Spouse’s Grieving Heart , Alan D.Wolfelt , mlangizi wa anthu amene akuvutika ndi cisoni analemba kuti : “ Cisoni ‘ sicipola ’ mmene munthu angapolele akadwala . ” Kukhumudwa Tingacitenji kuti ‘ tizifotokoza bwino mau a coonadi ’ ? Cimene cimaonetsa kuti munthu ni wacikulile kuuzimu si kuculuka kwa zaka zake ayi , koma kuopa kwake Yehova na kukhala wokonzeka kumvela malamulo ake . — Ŵelengani Salimo 111 : 10 . Iye anabadwa na matenda a Down syndrome , * ndipo tinali kuganiza kuti posapita nthawi adzamwalila . Filip ndi Ida anafotokoza zimene anacita kuti athandize ophunzila Baibulo kupita patsogolo . Komabe , Naomi anali wofunitsitsa kupita kwao ku Isiraeli . Gene Smalley Komabe , boma la padziko lonse limene limaganizila anthu likhoza kuonetsetsa kuti anthu onse ali ndi zimene amafunikila . Zoonadi , mfundo za m’Baibo n’zothandiza kwambili maka - maka masiku ano . Kwa nthawi yaitali anthu akhala mu ukapolo wa ucimo na imfa , ndipo akumana na mavuto ambili - mbili , cakuti ayamba kuwaona kuti ndiye umoyo . Timadziŵa bwanji kuti zimene timaona zingakhudze mtima wathu ? Yehova anamvetsela mapembedzelo a Rakele , ndipo anam’dalitsa mwa kum’patsa ana . ( 2 Pet . 3 : 9 ) Ganizilani mmene anayankhila kupitila mwa angelo pamene Abulahamu na Loti anali kumufunsa mafunso . 3 : 1 , 4 ) Okalamba ambili amayesetsa kukhala ndi moyo wosalila zambili . Tingacite zimenezi mwa kucilikiza mfundo zolungama za Mulungu , kusakhala mbali ya dziko la Satanali , ndi kuika zinthu za Ufumu patsogolo . ( Mat . 6 : 33 ; Yoh . Pali anthu ena ocepa amene Yehova anawasonyeza cikondi cake cosatha m’njila yapadela kwambili . Tiyenela kulimba mtima , kumvela Yehova ndi kum’dalila . Kodi izi ziyenela kutivutitsa maganizo kapena kutipangitsa kuganiza kuti Yehova analanga Azariya popanda cifukwa ? N’ciani cinathandiza Yesu kucita zinthu mokoma mtima ? 27 : 57 . Kodi banja lake linalila malilo a kholo lodzikonda limeneli ? N’nadabwa ngako ! Delphine , amene tam’chula m’nkhani yapita anati nkhawa ndiye zinalengetsa kuti azimwa moŵa kwambili . M’pomveka kuti makolo acikhristu safuna kuti mwana wawo abatizike asanafike poti n’kudzipeleka moyenela kwa Mulungu . Alangizi a sukuluyo anali kuphunzitsa mwaluso . Conco , m’madela ambili , abale a mitundu yosiyana sanali kusonkhana pamodzi poyopa kuti Nyumba ya Ufumu idzawonongedwa . Baibo imakamba kuti cikhulupililo ni “ ciyembekezo cotsimikizika ca zinthu zoyembekezeledwa . ” Acikulile naonso angapindule ndi zofalitsa zimenezi . Tiyeni tikambilane ena mwa mapindu a pemphelo . ( Ŵelengani Deuteronomo 22 : 5 . ) 3 , 4 . ( a ) Kodi mtumwi Petulo anaonetsa bwanji kuti ubatizo ni wofunika kwambili ? Ndipo miyambi yake inakhala mbali ya Baibo . Ngakhale pamene ndinabatizidwa , ndinafunika kuyesetsa kuthetsa mkwiyo wanga . Nanga bwanji inuyo ? Palinso nkhani zothandiza kwa anthu okwatilana , acinyamata , ndi aja ali ndi ana aang’ono . Ndani amaona nchito imene mlembi amakhala nayo posonkhanitsa malipoti a utumiki wa kumunda ? Kucita zimenezi kudzatilimbikitsa kutsanzila cikondi ca Yehova mwa kuwathandiza . Ndinali kuŵelenga kwambili mabuku olembedwa ndi akatswili a ku Germany a nzelu za anthu , makamaka amene amafotokoza cifukwa cake anthufe tinakhalapo . Kukhulupilila malonjezo a Mulungu kunalimbikitsa Abulahamu kucita cifunilo ca Mulungu . Sisera analamula mkaziyo kuti kukabwela munthu aliyense womufunafuna , asamuulule . ‘ Nifuna kukhala munthu wabwino , mwamuna kapena mkazi wabwino . ’ Pokamba ndi anthu , sikuti Yehova anali kugwilitsila nchito Ciheberi nthawi zonse . ( a ) Abulahamu anaonetsa bwanji kuti anali ndi cikhulupililo cosagwedela m’malonjezo a Mulungu ? Iye atasintha maganizo ake omenya nkhondo , anayamba kumanga mizinda m’zigawo za fuko la Yuda na Benjamini zimene anali kulamulila . Tifunika kupempha mzimu wa Mulungu . ( Ŵelengani Machitidwe . 20 : 20 , 21 , 24 , 35 . ) “ Adzadziguguda pacifuwa cifukwa ca cisoni . ” Conco , anawalimbikitsa kuti : “ Dzipezeleni mabwenzi ndi cuma cosalungama , kuti cumaco cikatha , [ Yehova na Yesu ] akakulandileni m’malo okhala amuyaya . ” Kucita zimenezo kunathandiza kwambili . Kodi Asa anazindikila kumene mtendele umenewo unacokela ? Nawonso madalitso a dipo ni a muyaya . Kodi mungacite ciani kuti makolo azoloŵele mwamsanga ndi kusintha kwa zinthu ? Iye anawapha onse . “ Ndife anchito anzake a Mulungu . ” — 1 AKOR . Ciyembekezo cathu cozikika pa Baibo cingatithandize kucepetsa nkhawa . 4 : 9 . N’cifukwa ciani ngakhale amkhalakale m’coonadi amafunikila cilimbikitso ? Koma pamene anasintha khalidwe lake , anayamba ‘ kufuna kudziŵa zinthu ’ ndipo anapempha thandizo kwa akulu . N’ciani cingatipangitse kusiya kuyamikila zonse zimene Yehova waticitila ? Koma imatilangizanso kuzikonda na kuziseŵenzetsa mu umoyo wathu wa tsiku na tsiku . Takamba conco cifukwa Baibo imaonetsa kuti Yesu Khiristu ndiye anali woyamba kuukitsidwa kuti akakhale kumwamba . — Yohane 3 : 13 . Nabala ndi onse a m’nyumba yake anali kudzalangidwa cifukwa ca kupanda nzelu kwake . — 1 Sam . Mwana wa Mulungu anapatula nthawi yothandiza anthu kukhala na cikhulupililo colimba . Kodi iye anamuumila mtima monga mmene Afalisi anali kucitila ndi anthu odwala matendawa ? 5 : 17 - 19 . Adzakhalanso odzikuza , ndi aukali . Nanga amakonzekela bwanji kuti akwanitse utumiki umenewu ? Ndipo lemba la Aroma 12 : 19 limaticenjeza kuti : “ Musabwezele coipa , . . . pakuti malemba amati : ‘ “ Kubwezela ndi kwanga ndidzawabwezela ndine , ’ watelo Yehova . ” Ofesi ya nthambi imene inali ku Blantyre inalandidwa , ndipo amishonale anapitikitsidwa komanso Mboni za kumeneko , kuphatikizapo ine ndi Lidasi , tinaikidwa m’ndende . Tiyenela kuika Yehova patsogolo mu umoyo wathu Ngati tiyang’anitsitsa Yesu ndi kum’tsatila mosamala kwambili , tidzakhala ndi cikhulupililo colimba ( Onani ndime 15 ) Komabe , Mose anali ndi cidalilo cakuti Mulungu akanasintha zinthu . Kuti zimenezi zitheke , pali zinthu zitatu zimene tiyenela kucita . Nanga n’ciani cingatithandize kusinkhasinkha nthawi zonse ndiponso mosangalala ? Pakuti Yesu anati : “ Munalandila kwaulele , patsani kwaulele . ” Kodi mumapemphela kaŵilikaŵili kwa Yehova ? N’zoona kuti makonzedwe amenewa anali mbali ya pangano la Cilamulo , limene linaloŵedwa m’malo na pangano latsopano pa Pentekosite wa mu 33 C.E . Mungayeseko njila ina . Kodi Baibo imati n’ciani camtengo wapatali kuposa golide na siliva ? A Zimba : Ndi mau akuti ufumu . 9 : 6 , 7 . Kapepala ka Uthenga wa Ufumu Na . 30 m’Cituvalu Makhalidwe athu . — 1 Akorinto 6 : 9 , 10 . ( Chiv . 7 : 14 - 17 ) Ndipo palibe mtsogoleli wina aliyense amene angalonjeze zimenezo . Nanga tingatsimikize bwanji kuti nchito yathu yolalikila ikukwanilitsa zimene Yesu anakamba ? Mmene Yehova Amayandikilila kwa Ife Moona mtima , amapenda mmene mikhalidwe yake ilili . Kuti buku likhale lothandiza ndiponso lofunika kwambili kwa anthu , liyenela kukhala losavuta kumvetsetsa . Iye anati : “ Inu eni mukudziŵa bwino kuti tsiku la Yehova lidzabwela ndendende ngati mbala usiku . ” Pamene tsiku la Yehova “ likuyandikila , ” kulimbikitsana kudzakhala kofunika ngako . ( Aheb . Ngakhale kuti Sauli anali akali msilikali wamphamvu , Yehova analeka kumukonda cifukwa sanamvele malangizo ake . Dziko lina ku Asia linacitila lipoti kuti m’zaka 10 zapitazi , acinyamata ambili kumeneko ndi amene anapalamula milandu ikuluikulu . 16 : 6 , 7 ) Koma kodi anafunika kupita kuti ? Roger , tate wa ana aŵili ku South Africa anafotokoza kuti , “ ana athu amapeza zinthu zimene sitinazione m’Baibulo . ” ( Yohane 8 : 44 ) Iye anayambitsa kupanduka m’munda wa Edeni . Mdulidwe unali kucitidwa pa tsiku la namba 8 kucokela pamene mwana wabadwa . Pelekani zitsanzo . ( b ) Kodi fanizo limeneli likutiphunzitsa ciani ponena za Yehova ndi Yesu ? 25 Kodi Mumaona Kufunika Kophunzitsa Ena ? N’cifukwa ciani tili ndi cidalilo cakuti tidzapambana panchito yathu yocitila umboni ? Yehova sadzaiŵala kudzipeleka kwa anthu okhulupilika amenewa . Kodi nchito yanga imapindulitsa bwanji anthu ena ? ’ ( Luka 22 : 32 ) Mofanana ndi Mose , muziganizila zotsatilapo zaucimo , mwai wotumikila Yehova ndi ciyembekezo ca moyo wosatha . Masiku ano , ngakhale ena akambe mau oipa okhudza utumiki wake , iye amakhalabe wosangalala cifukwa codziŵa kuti akucita zimene angakwanitse kuti akondweletse Yehova . Tisakhalile kupeza anzathu zifukwa . Pamene anthu anamvetsetsa ulosi wa pa Genesis 3 : 15 , anakhala na ciyembekezo cakuti m’tsogolo “ njoka yakale ija , ” Satana Mdyelekezi , adzawonongedwa pamodzi na nchito zake zonse zoipa . — Chiv . N’cifukwa ciani anthu a Yehova afunika kukhala oyela ? ( Aroma 14 : 21 ) Akhristu ena angadabwe kapena kukhumudwa ngati adziŵa kuti wina mumpingo ali na mfuti yodzitetezela kwa anthu ena . Zaka mahandiledi pambuyo pake , Yesu anakhazikitsa Mgonelo wa Ambuye pa Nisani 14 , 33 C.E . Baltasar Perla , Jr . ( b ) Tingaonetse bwanji pa zocita zathu za tsiku na tsiku kuti tinadzipelekadi kwa Mulungu ? M’malomwake , kaŵili konse Yesu anamvela Atate wake akukamba kuti : “ Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa , amene ndimakondwela naye . ” ( Mat . 5 , 6 . ( a ) N’cifukwa ciani kusinkha - sinkha n’kofunika ? 8 : 44 - 47 ) Nanga tingacitenji kuti tisagonje ? Panthawiyo n’kuti kwa milungu ingapo m’mbuyomo , tinazindikila kuti omasulila mabuku akukumana ndi mavuto . Ida wa zaka 19 , wakhala akuvutika na maganizo odziona monga wosafunika . Kodi anali kugwilitsila nchito zizindikilo zotani ? Ine na mkazi wanga tinali kukhala olema komanso opanikizika maganizo . Yehova analenga zinthu za mitundu yosiyanasiyana n’colinga cakuti tizisangalala . ( Sal . ( 1 Pet . 2 : 21 , 23 ) Tifunika kuganizila kwambili citsanzo ca Khristu maka - maka ngati ena atikhumudwitsa kapena aticitila zinthu zopanda cilungamo . Conco , ndinaganiza zosintha umoyo wanga ndipo ndinayamba kuphunzila Baibulo . Komabe , banjalo linafuna kuti Rabeka akhale nao kwa masiku ena 10 . N’ciani cawathandiza kusintha ? Muziganizila zimene abale ndi alongo anu akufunikila , kaya ndi thandizo lacindunji , citonthozo , kapena cilimbikitso ca m’Malemba Ayenela kuti anatenganso anthu ena amene anatsala mu ufumu wa Isiraeli wakumpoto . Mafumu ocokela mu mfuko la Yuda anali kulamulila mu ufumu wa mafuko aŵili amenewa . Nchito imeneyi imakamba za uthenga wabwino wakuti posacedwapa “ mapeto adzafika ” kudzela mu Ufumu wa Mulungu . Iwo anacita zinthu mogwilizana , ndipo palibe amene anali kucita za mumtima mwake . Ganinilaninso cimwemwe cimene iye adzakhala naco , akadzadziŵa kuti mbili yake inalembedwa m’buku la m’Baibo lodziŵika na dzina lake . — Rute 4 : 13 ; Mat . Yehova adzanikhululukila . ’ Abale , alongo , ndi acicepele ambili - mbili adzipeleka mwa kucita mautumiki osiyana - siyana a nthawi zonse , monga upainiya , kutumikila pa Beteli , ndi kuthandiza pa nchito yomanga Nyumba za Ufumu . Ena amagwila nchito yodzipeleka pa misonkhano yadela ndi yacigawo . Makolo , Thandizani Ana Anu Kukhala na Cikhulupililo , Sept . ( Yak . 1 : 13 ) “ Mdani wanu Mdyelekezi , ” ndi amene amacititsa mavuto ambili . Siticilikiza mbali iliyonse m’nkhani za ndale . M’malo modalila anthu kuti ndiye adzatipulumutsa , timaonetsa kuti ndise anzelu ngati tidalila Mlengi wathu , amene ali na mphamvu zokwanilitsa malonjezo ake onse . 51 : 12 ; Sal . 60 : 13 . Onani Buku Lothandiza Pophunzila Mau a Mulungu , Cigawo 16 . NYIMBO : 20 , 119 Mwina Akristu ena anadabwa cifukwa cake anthu amenewo analoledwa kukhalabe mu mpingo . Kodi kuganizila zinthu zimene Yehova amaticitila kungatithandize bwanji ? Sara Iye anaona kuti afunika kusintha kwambili khalidwe lake . ( 1 Akor . Yehova anatidalitsa mwa kutithandiza kupeza nchito yophunzitsa ya maola ocepa pa sukulu ina yake . ( Yohane 14 : 2 , 3 ; Afilipi 3 : 20 , 21 ) Anthu amene adzapita kumwamba “ adzakhala ansembe a Mulungu ndi a Kristu , ndipo adzalamulila monga mafumu limodzi naye zaka 1,000 . ” — Chivumbulutso 20 : 6 . Tifunika kuika patsogolo zinthu zofunika kwambili kuti tikwanitse kukhala na umoyo wosalila zambili . Kodi mungakonzekele bwanji kuti mudzakhale mtumiki wanthawi zonse ? Conco , kaya takhala tikutumikila Yehova kwa zaka zingati , pali zinthu zina zambili zimene tingaphunzile zokhudza makhalidwe ake . Mwacitsanzo mungaphunzitseko acinyamata zinthu zimene mwaphunzila kwa Yehova . “ CIYEMBEKEZO . . . Iye sanacitile nsanje Yaeli n’kulephela kumutamanda , koma anakondwela kudziŵa kuti mau a Yehova akwanilitsidwa . Inde , tifunika kukhala na mtima wofuna kuphunzila mfundo zambili za coonadi . ( Amosi 5 : 14 , 15 ; 1 Pet . Koma tsogolo la dziko silidalila pa zocita za anthu . N’ciani cingakuthandizeni kupitiliza kukhala wacangu mu utumiki ? Cacinayi , Yehova safunika kudziŵilatu ciliconse cimene cidzaticitikila . Kodi zimenezi zimatipindulitsa bwanji ? 32 : 4 ; 2 Akor . TSOPANO ndi nthawi yakuti Timoteyo acoke panyumba ndi kusiya makolo ake . Maganizo ake onse ali pa utumiki umene akuyembekezela kucita . Koma “ Woyesayo ” ndi Mdyelekezi . ( Mat . Iye anali kucondelela Mulungu m’pemphelo kuti athandize Ayuda kulabadila uthenga wa Ufumu . Izi n’zimene iye anacita kwa anthu oyambilila atangowalenga . Koma kukhala osiyana ndi dziko ndiponso kupewa makhalidwe oipa ndi zinthu zina zimene zingaononge ubwenzi wanu ndi Mulungu , kudzakuthandizani ‘ kugwila mwamphamvu moyo weniweniwo . ’ Kodi tingaphunzile ciani tikaona zimene zinawathandiza kukhala mabwenzi a Mulungu ? Ngati ndinu wodzicepetsa ndipo mumapewa kudzikonda , mumaphunzitsa ana anu kukhala ofunitsitsa kuthandiza ena . Ndidziŵa kuti Baibulo lili ndi mphamvu zothandiza aliyense kuti akhale ndi moyo wabwino ndi waphindu . Wacinyamata wofikapo mwakuuzimu angakhale wokhulupilika ngakhale pa nthawi yovuta Caka ciliconse , fodya umapha anthu pafupifupi 6 miliyoni . Aisiraeli atatsala pang’ono kuloŵa m’Dziko Lolonjezedwa , Yehova anawauzanso malamulo ake . Mwacitsanzo ofalitsa ena anali amanyazi . Ena anapita popanda mapepala acilolezo ndipo sanapeze nchito . Kodi nkhani yake inayenda bwanji ? Mlongo wina wa ku Asia , dzina lake Rebecca , anakamba kuti iye ndi banja lake anatsatila mfundo ya pa Mateyu 6 : 33 ndi ya pa Miyambo 10 : 4 . Pogwilako mau a m’magazini yochedwa The Golden Age , m’bale Arthur Willis anati : “ Khote - khote ngwanjila , palinga mtima mpomwepo . ” Chulani cinthu cimodzi cimene cimapangitsa anthu kukhala apamwamba kuposa nyama . N’ciani cinawathandiza ? Kodi anthu ena anapindula bwanji ndi maphunzilo a Yesu akuuzimu ? Conco , mukawaitana ku cakudya muziwafunsa ngati angakonde kulaŵa zakudya zanu , kapena ngati pali zakudya zina zimene sangakonde . Ngati mwamuna na mkazi ni osakhulupilika m’banja , akakumana na mavuto , amathamangila kukamba mau monga akuti , ‘ Sindise oyenelelana ’ ndipo amafuna - funa njila zothetsela cikwati . Ndipo panthawi ina anati , “ Palibe amene amafika kwa Atate osadzela mwa ine . ” Kyung - sook , amene amakhala ku Asia , anali kucita upainiya ndi mwamuna wake kwa zaka zoposa 20 . 13 : 7 , 17 . ( b ) Ni anthu ati amene Yehova amakondwela nawo ? YESU anali kukonda kukamba za Ufumu wa Mulungu . Tifunika kum’dziŵa bwino Mulungu amene analemba Baibo . Pokamba ndi Mose na Aroni , Yehova anati : “ Amuna inu munapandukila malangizo anga . ” ( Num . Conco , ndisakutaileni nthawi . Tifunikanso kuphunzila zimene tiyenela kucita ena akatilakwila . Nsanja ya Mlonda yacingelezi ya September 15 , 1958 , inacenjeza abale ndi alongo kuti sayenela kulola zipangizo zamakono kuwasokoneza potumikila Yehova . Kodi mungaonetse bwanji kuti mufuna kukhala cimodzi mwa “ ziwalo za thupi limodzi ” ? Kodi n’koyenela Mkhristu kukhala na mfuti yodzitetezela kwa anthu ena ? Komabe , Mulungu sapeleka mzimu wake kwa anthu amene sadalila thandizo lake . Pa cifukwa cimeneci , iwo amalephela kuimvetsetsa . Popeza sitingamvele Mulungu akamba naise mwacindunji , timamvela iye mwa kuŵelenga na kucita zimene Mau ake Baibo amakamba . — 1 Yohane 5 : 3 . Nyanja . Onani Buku Lapacaka la Cingelezi la mu 1988 , mape . Buku la Coonadi Tinali kuonanso kukongola kwa mwezi ukawala usiku makamaka ngati waunika pa nyanja . Koma n’nali kukondwela ngako na nchito yolalikila . Baibulo imakamba kuti Yehova anapanga munthu wangwilo kucokela “ kufumbi lapansi , ” kapena kuti kudothi . ( b ) Ndi udindo wotani umene a “ nkhosa zina ” ali nao ? Nawonso makolo acikhristu afunika kukhala olimba mtima . Koma poyamba amayi ake anali kumudela nkhawa . Tikhulupilila kuti palibe amene anakhumudwa ndi colakwa cimene Petulo anacita . A Mboni za Yehova a kudela lanu , adzasangalala kukuthandizani kuti mupindule na thandizo lacikondi la angelo a Mulungu amphamvu . Philip anawagwilitsila nchito malangizowo , ndipo tsopano akutumikila monga mkulu . — Miy . Pemphelo si njila yongofuna kupempha thandizo . Tingawathandize bwanji anthu amene ali na maganizo akuti munthu akhoza kudziŵa zabwino na zoipa popanda kukhulupilila Mulungu ? Pamene anali wacinyamata , Yesu anapeleka citsanzo cabwino cifukwa anali kukonda misonkhano . Ngakhale pambuyo pobatizidwa , Kevin anafunika kupitiliza kusintha umunthu wake kuti akhale Mkristu wabwino . Zimenezi zidzalimbitsa cikhulupililo canu mwa Mulungu , ndipo ubwenzi wanu ndi iye udzalimba kwambili . ( Ŵelengani Aroma 2 : 14 , 15 . ) 3 Mphatso Yopambana Zonse Mlongoyo na ana ake anali kuuka kuseni - seni kukacita pisiweki yolima m’munda wa thonje kuti apeze ndalama zakuti nikayendele ku New York . Cimene munthu wina angaone kuti n’cabwino koposa , kwa wina sicingakhale conco . M’nkhani yotsatila , tidzaphunzila zambili zokhudza Baibulo limeneli , ndiponso mmene likumasulidwila m’zinenelo zina . Popeza kuti makolo anga anali kukhala ku South America , ndinali kuzisamalila ndekha . Iwo amamasulilanso mabuku m’zinenelo zina zambili zosachuka , koma zimene zimalankhulidwa ndi mamiliyoni a anthu . Tifunika kupitiliza kufunafuna Ufumu coyamba ndi cilungamo ca Mulungu mwa kutengako mbali panchito yolalikila uthenga wabwino . — Mat . Mu umoyo wanga wonse , nakhala na mwayi woyendela anthu a Yehova m’maiko 33 . Pambuyo pophunzitsidwa za nchitoyi kwa wiki imodzi , tinapita ku Scotland kukatumikila m’dela limene anatigaŵila . Tingacitenji kuti ‘ tileke kucita zosalungama ’ pankhani yoleka kugwilizana ndi anthu oipa ? Buku lina limanena kuti atsogoleli a maiko a ku Ulaya ‘ sanali kudziŵa kuti zosankha zao zidzayambitsa mavuto a padziko lonse m’caka ca 1914 . ’ — The Fall of the Dynasties — The Collapse of the Old Order 1905 - 1922 . Mosakaikila , mumaonanso kuti ambili samvela makolo , ndiponso anthu oculuka amakonda kwambili zosangalatsa kuposa Mulungu . Baibulo limatiuza kuti : “ Ona munthu wosalakwa ndipo yang’anitsitsa munthu wolungama , pakuti tsogolo la munthu ameneyu ndi lamtendele . N’ndani amafunikila cilimbikitso ? Kodi tingaphunzilepo ciani pa funso limene Yesu anafunsa Petulo ? Anazindikilanso kuti munthu “ sangakwanitse kupilila ngati saŵelenga Baibo . ” Iye analimbikitsa abale ake kuti : “ Musalole kuti ucimo uzilamulilabe monga mfumu m’matupi anu okhoza kufawo kuti muzitsatila zilakolako zawo . ” Mu Ufumu wa Mulungu , anthu “ adzasangalala ndi mtendele woculuka . ” — Salimo 37 : 11 15 , 16 . ( a ) Kodi kukonda cuma kungakhale msampha kwa Mkhristu m’njila yanji ? Ndipo anamuuzanso kuti : ‘ Umu ndi mmene mbeu yako idzakhalile . ’ ” ( Gen . Kodi a “ nkhosa zina ” angapindule bwanji ndi fanizo la anamwali 10 ? Izi zionetsa kuti m’dziko mumafunika kukhala malamulo kuti munthu aliyense apindule na ufulu umene ali nawo . Nikalibe kuphunzila coonadi , n’nali na maganizo olakwika ponena za mmene mwamuna weni - weni afunika kukhalila . Kodi akulu ndi ofalitsa ena angathandize motani apainiya apadela ? Conco , mwacimwemwe ndi modzipeleka , iwo anayamba kugwila nchito yobwezeletsa kulambila koona ku Yerusalemu . Kodi amuna apaudindo ayenela kucita ciani akalandila malangizo a gulu la Mulungu ? ( b ) Kodi colinga ca Sukuluyi cakhala cotani kuyambila 2011 ? Iwo anakamba kuti Paulo akuyambitsa zoukila boma pakati pa Ayuda onse , akutsogolela gulu la mpatuko , ndi kuti akudetsa kacisi amene panthawiyo anali m’manja mwa Aroma . ( Mac . Yehova anam’dalitsa Hana cifukwa ca kudzimana kwake . Yesetsani kukulitsa cikondi canu pa abale . Ngati musinkhasinkha mmene Yesu anali kucitila zinthu ndi anthu mudzatha kuona bwinobwino makhalidwe osangalatsa a Mulungu ndipo mudzamuyandikila . Ndikucititsa msonkhano wokonzekela ulaliki pamene ndinali woyang’anila woyendela Kodi analeka kukhulupilila Mulungu wake , Yehova ? Cimakhala cosavuta kwa iwo kupewa mzimu wonyada , wodziona monga ofunika kwambili kapena olungama ngako . Kodi Akhristu apabanja ayenela kuona kuti kuseŵenzetsa ma IUD ni njila ya cilezi yogwilizana na Malemba ? Nthawi zambili , pa Ciŵelu na pa Sondo tinali kukhala kumeneko . Rudi anacita zinthu mwanzelu ndipo sanandipatsenso buku lililonse . Izi zikupangitsa kuti mphatso iliyonse yocokela kwa iye ikhale yamtengo wapatali . Pa cifukwa cimeneci , Yosefe anapempha wopelekela cikho kuti akafotokoze za iye kwa Farao . Mukacita zimenezi , mudzazindikila mwamsanga kuti mumafanana pa zinthu zina ngakhale kuti ndinu wosiyana mtundu . Paja cikhalidwe ciliconse cili na zabwino na zoipa zake . ( Yeremiya 10 : 23 ) Iye amaona anthu onse monga banja limodzi . Izi zingatheke mwa mphamvu ya mzimu woyela , umene timaupeza mwa kupemphela , kuphunzila Mau a Yehova na kuwasinkha - sinkha . Analeka kumvela malamulo a Yehova na kuyamba kulambila mafano . Ponena za “ wolamulila wa dzikoli , ” Satana Mdyelekezi , Yesu analonjeza kuti ‘ adzaponyedwa kunja tsopano . ’ Tikali kucitila zinthu limodzi , ndipo panopa timacitila upainiya limodzi . Kuonjezela apo , timakonda anzathu . Iye amadziŵa izi ife eni ake tikalibe kudziŵa . ( Afil . 4 : 19 ) Ngati covala cinacake cimene timavala cili pafupi kusila , amadziŵa kuti tifunikila cina . Pa cifukwa cimeneci , atumiki a Mulungu anali okhoza kulankhula ndi anthu osiyanasiyana , ndipo izi zinathandiza kuti uthenga wabwino ufalikile . Kuyankha mwacidule , Baibo imakamba kuti akufa ali kumanda , kuyembekezela kuukitsidwa . 11 : 35 . 2 : 15 ) Nanga ifenso tingatsatile motani malangizo a Paulo ? Kuti mudziŵe nthawi ndi malo amene kudzacitikila mwambo wosalipilitsa umenewu , mungafunse wa Mboni za Yehova kwanuko kapena mungapite pa webusaiti yathu ya www.jw.org . Kodi Satana angatikakamize kucita zinthu zimene sitifuna ? Tate wina ku Japan anavomeleza kuti , “ poyamba zinali zacilendo kuŵelenga mwa njila imeneyo . ” 106 : 1 . Sauli anafuna kuteteza dzina lake , ndipo zimenezi zinam’lepheletsa kulandila thandizo la kuuzimu . ( Yesaya 48 : 17 , 18 ) Tsopano umoyo wanga wakhala ndi colinga cimene ndinalibe poyamba . Comalizila , anthuwo atakhala ndi moyo , Yehova anawapatsa dziko kuti akhalemo . Ndiye cifukwa cake Yehova anali kumukonda kwambili . M’fanizoli , atate a mwana uja anali ndi ciyembekezo cakuti mwana wao adzabwelela . Zili monga anthu amene akhala pafupi na msewu waukulu umene mumapita mamotoka ambili . Kodi iwo anabwelele ku dziko lawo kuti akacite zofuna zawo cabe ? Komabe , anthu ake anafunikila kucitapo kanthu mwa kupatukana ndi anthu osakhulupilikawo . Koma tikumbukile kuti zimenezi n’zongoyelekezela cabe . Nanga ife tonse , kuphatikizapo Akhristu acicepele , tingamutsutse bwanji ? Adzacita zimenezi mu umoyo wake wonse , ngakhale kwamuyaya . — Aroma 11 : 33 , 34 . ( Ŵelengani Salimo 147 : 5 . ) Kodi tingacite ciani kuti tizikhululukilana msanga ? 15 : 14 , 15 . Mau a Mulungu amaletselatu khalidwe la kukopana . ( Genesis 37 : 3 ) Covala cimeneco cimachedwa mkanjo wamizelemizele kapena kuti wamaŵangamaŵanga . Komabe , thandizo limene amapeleka silicotsela anawo udindo wosamalila makolo ao mmene angathele . MUZILEMEKEZA OKALAMBA NDI MAU OLIMBIKITSA Kuti aigule , anafunika kugulitsa zonse zimene anali nazo . M’malo mocita zimene akuuzani cabe , muzicita zambili kuposa pamenepo . Kuyambila m’nthawi ya atumwi , ophunzila odzozedwa akhala akupatsidwa matalente , kutanthauza nchito yolalikila . Kodi mumaona kuti ndi mwai wanu kugwilila nchito limodzi ndi Yehova pokongoletsa ‘ malo oikapo mapazi ake ? ’ Motelo , muzifotokoza bwino mmene aliyense angaseŵenzetsele mfundo zimene mwaphunzila pa kulambila kwa pabanja , kuti nonse mupindule . — Sal . Kodi zokamba zanu zimaonetsa kuti mumaika maganizo anu pa za mzimu kapena za thupi ? Kuti mpingo ukhale woyela ndi wogwilizana , kodi akulu afunika kucita motani ? Umu ndi mmene kuwala kozungulila pamalopo kunali kuonekela . Conco , n’nali wotangwanika na kagulu ka anyamata kocilikiza Cikomyunizimu . wamphamvu ? Iye anadzimana zambili kuti akhale wolambila woona . Kudela lina la mzindawu kumene kunaonongeka kwambili , anthu anayamba kutenga katundu wa anthu a kumeneko omwe anali kale pa vuto losoŵa magetsi ndi zinthu zina . Koma anzanga a ku nchito sanamvetsetse cifukwa cake n’naleka zinthu zimenezi . Pamene tilemekeza akulu mumpingo , tifunika kutsatila mfundo za cilungamo ndi zothandiza zopezeka m’Mau a Mulungu . Umenewu ndi mwai wamtengo wapatali . Adzapitilizabe kuwatsogolela mpaka pa cionongeko ca dongosolo ili la zinthu ndi kuwaloŵetsa m’dziko latsopano . — Ŵelengani 2 Petulo 3 : 7 , 13 ; Chivumbulutso 7 : 17 . Baibulo limatiuza kuti : “ Pitilizani kudziyesa kuti muone ngati mukadali olimba m’cikhulupililo . Kuwonjezela pa izi , tinaona maphunzilo athu a Baibo akupita patsogolo . Kukhala na zolinga zauzimu na kuzikwanilitsa kwathandiza ana athu kuti asagonje ku zokopa za m’dziko la Satanali . Kwawathandizanso kuika maganizo awo pa kutumikila Yehova . ” Takamba conco cifukwa ena mwa alendowo anauza Yohane za cikondi na cikhulupililo ca Gayo . — 3 Yoh . 3 , 6 . Pamene mupitiliza kuphunzila Baibo mwakhama , mudzapeza mfundo zambili zothandiza . M’bale wina wa ku Mexico , dzina lake Daniel , anafunika kusankha kuti adzakhala wokhulupilika kwa ndani . Kukamba zoona , kucita zimene Yehova amafuna , nthawi zonse kumabweletsa madalitso . Munthuyo anali kudziŵa kuti Yesu anali ndi mphamvu zotha kumucilitsa , koma sanali kudziŵa ngati Yesu anali wofunitsitsa kumuthandiza . Kodi Robert ndi mkazi wake anacita ciani pamene anali ndi zaka za m’ma 50 ? Tinapemphela pamodzi ndi kupita kukagona . 3 , 4 . ( a ) Ndi mzimu wotani umene wafala pakati pa acinyamata masiku ano ? Pa utumiki wake , Yesu anaonetsa kuti anali wozindikila ndi wacifundo . Pakuti anthu adzakhala odzikonda , okonda ndalama , . . . osakhulupilika , osakonda acibale ao , osafuna kugwilizana ndi anzao , onenela anzao zoipa , osadziletsa , oopsa , osakonda zabwino , aciŵembu , osamva za ena , odzitukumula ndiponso onyada . ” — 2 Timoteyo 3 : 1 - 4 . Kodi Yehova amalankhula nafe bwanji ? Ngati mwamuthandiza mwa njila imeneyi , mudzaona kuti wophunzila Baibulo adzayamba kusangalala pophunzila Mau a Mulungu payekha . Tikaganizila zimene tacita pa umoyo wathu , timavomeleza na mtima wonse kuti taonadi cisomo ca Yehova m’njila zambili - mbili . ULAMULILO WA YEHOVA PAMBUYO PA CIGUMULA Onetsetsani kuti wodwalayo na bedi yake n’zaukhondo . Amaona kuti alibe nthawi yophunzitsa ena . Kaya ciyembekezo canu ndi cakumwamba kapena ndi ca padziko lapansi , cidzakwanilitsidwa kokha ngati mumakhulupilila Yehova Mulungu , Yesu Kristu , ndi dipo . 14 Kucelezana ni Khalidwe Lofunika Kwambili Ngakhale kuti oweluza amene anasankhidwa anali amuna anzelu ndi aluso , io sanaloledwe kuweluza mogwilitsila nchito nzelu zao kapena luso lao . Ayuda ambili amapeleka pempheloli tsiku lililonse m’maŵa ndi m’madzulo pofuna kuonetsa kudzipeleka kwawo kwa Mulungu . N’cocitika citi cimene cidzagwilizanitsa anthu oculuka mu 2018 ? 13 : 35 ) Mboni zinatsatilanso kwambili malangizo amene mtumwi Paulo anapeleka kwa Akristu a ku Korinto . — Ŵelengani 2 Akorinto 10 : 3 , 4 . Kapena sembe munayamba kuyelekezela mipanda yolimba ya Babulo ndi mpanda wogumuka - gumuka wa Yerusalemu , wokhala na mipata ikulu - ikulu m’malo amene munali zipata ndi nsanja za alonda ? Izi n’zimene Sophie , amene anali ndi luso lovina anasankha . Mulungu sayembekezela kuti tizikamba cinenelo cina cake n’colinga cakuti tim’dziŵe ndi kudziŵa zolinga zake . ( 2 Maf . 22 : 11 ; 23 : 1 - 23 ) Cifukwa cakuti Yosiya ndi atsogoleli ena okhulupilika anatsogoleledwa ndi Mau a Mulungu , iwo anali ofunitsitsa kusintha ndi kumveketsa bwino malangizo amene anali kupatsa anthu a Mulungu . MUSAMAKHAZIKIKE PA ZINTHU ZOKUVUTITSANI MAGANIZO . 3 : 18 ) Kuti anthu atsimikize kuti Yesu waukadi , anavala thupi laumunthu ndi kuonekela kwa anthu . Bodza limenelo linafala m’nthawi ya Yobu , ndipo lafalanso masiku ano . — Yobu 4 : 18 , 19 . Kodi Tiyenela Kupemphela kwa Yesu ? Tingacite zimenezi pasadakhale , ndi kuwayamikila pa ciitano cao . Koma nayenso nthawi ina anapanga zosankha mosaganiza bwino . Komabe , Munthu amene tiyenela kukhala naye paubale wolimba kuposa onse ndi Mlengi wathu Wamkulu . — Mlal . Kucokela pamene kapolo wokhulupilika anaikidwa mu 1919 , iye wakhala akukonzela anthu a Mulungu cakudya cauzimu ( Onani palagilafu 10 , 11 ) Timacita zimenezi mwa kukamba nao kapena kucita zizindikilo ndi manja . [ Mau apansi ] Pofotokoza Mau a pa Ekisodo 3 : 14 , katswili wina wolemba Baibulo anati : “ Palibe cimene cingalepheletse Mulungu kukwanilitsa cifuno cake . . . 15 : 28 . Nkhani ziŵilizi zidzaonetsa mmene Yehova amatithandizila ndi dzanja lake lamphamvu kuti tipilile mavuto . PA December 26 , 2004 , civomezi camphamvu kwambili cinagwedeza cilumba ca Simeulue . Cilumba cimeneci cili kumpoto koma cakumadzulo kwa mzinda wa Sumatra ku Indonesia . ( Gen . 1 : 26 - 28 ) N’zosangalatsa kwambili kuti Yehova anatilenganso ndi makhalidwe amene amatithandiza kumutsanzila . — Aef . Oweluza anali kugamula mlandu pokhapo pakakhala umboni wokwanila . Mpake kuti anthu ambili anali kukonda kukhala pafupi ndi Yesu cifukwa anali kudziŵa kuti adzawatsitsimula . N’cifukwa ciani kuŵelengela anthu malemba mu ulaliki pakokha si kokwanila ? Ndiyeno , kuukila kumeneku kudzayambitsa Aramagedo , imene ndi mbali yotsiliza ya “ cisautso cacikulu . ” ( Mat . 24 : 21 ; Ezek . 1 : 21 ) Ndiyeno munazindikila kuti Atate wathu wakumwamba amene ndi wacikondi sali kutali ndi ife ndipo amatiganizila . ( 1 Akor . 16 : 2 ) Conco , munthu aliyense , kaya wolemela kwambili kapena wosauka kwambili , anali na mwayi wocita zopeleka . — Luka 21 : 1 - 4 . ( Miy . 30 : 8 , 9 ) Mwacionekele , mudziŵako anthu ena amene amadalila cuma cawo m’malo mokhulupilila Mulungu . Paulo anayelekezela Cikumbutso ndi cakudya cimene timadya ndi ena , ndipo anacenjeza anthu amene amadya zizindikilozo kuti : “ Sizingatheke kuti muzimwa za m’kapu ya Yehova komanso za m’kapu ya ziwanda . Sizingatheke kuti muzidya patebulo la Yehova komanso patebulo la ziwanda . ” ( 1 Akor . Onse m’banja maka - maka makolo ayenela kuyesetsa kuona zinthu moyenela ndi kukambilana momasuka . Nchito yolalikila uthenga wa Ufumu kwa ena imatipatsa mwayi wapadela wocitila anthu “ onse zabwino . ” Ngati n’conco , muziyesetsa kuseŵenzetsa mfundo za Yehova m’cikwati canu . Baibo ya King James Version inakhala imodzi mwa mabaibo a Cizungu ofala ngako , ndipo inakhudza kwambili cinenelo ca Cizungu . N’ciani cingathandize kuti cikwati cikhale colimba ? ( b ) N’cifukwa ciani tiyenela kuyembekezela kuti Yehova adzayankha tikapempha cikhulupililo coonjezeleka ? Kutanthauza kuti mlungu uliwonse panali kubatizidwa anthu 5,300 . Ndiyeno , amayi ake amuuza kuti : “ Iwe Johnny , leka kuseŵeletsa bola m’nyumba ! Delphine amene tam’chula kuciyambi anati : “ Mwana wanga wa zaka 18 atamwalila , n’nali na cisoni cacikulu cakuti siinali kukhulupilila kuti nidzapitiliza kukhala na moyo . Zoonadi , Davide anadziŵa kuti anafunika kuyembekezela kuti alandile madalitso a Mulungu . Mwacitsanso , ganizilani nkhani za m’Baibo za pa Genesis 20 : 2 - 7 ndi Mateyu 26 : 31 - 35 . Ngati ndi kotheka , khalani mwamtendele ndi anthu onse , monga mmene mungathele . ” Kodi Mulungu anapanga makonzedwe otani kuti dziko lapansi lidzaze ndi ana ake aumunthu ? Abale na alongo amene akutumikila m’dzikoli anacokela ku Canada , Czech Republic , France , Germany , Guadeloupe , Luxembourg , New Caledonia , Sweden , Switzerland , United Kingdom , na United States . Koma kodi tingacite ciani kuti iye atidziŵe ? Ndipo atapemphela , “ sanakhalenso ndi nkhawa . ” Kodi kuukitsidwa kwa Yesu kunawakhudza bwanji ophunzila ake ? Yehova anauza Eliya kuti : “ Kodi waona mmene Ahabu wadzicepetsela pamaso panga ? Ulosiwo unakambanso kuti anthu amene amalambila Mulungu m’masiku ano otsiliza adzagwilizana ndi kukhala mtundu umodzi . ” Iye anali wopanda colakwa pakati pa anthu a m’nthawi yake . 3 Kodi Mumalandila “ Cakudya pa Nthawi Yoyenela ” ? Ena amakondwela na nchito imene amagwila , maseŵela , kapena zosangalatsa . 6 : 25 ) Rahabi anali ndi cikhulupililo , ndipo iye anaopa Yehova ndi kulemekeza anthu ake . Iye anati , “ Kuona mmene mipingo na tumagulu tukuculukila m’madela akutali , kumanipatsa cimwemwe cacikulu . Komabe , maboma a anthu amalephela kuphunzitsa anthu makhalidwe abwino ndipo sangakwanitse kutelo . Kodi mudzapitilizabe kukonda Yehova ndi mtima wonse ? Ambili anali kufuna kupita ku yunivesite n’colinga cakuti akapeze nchito yabwino . N’cifukwa Ciani Tifunika Kumvetsetsa Baibulo ? N’ciani cofunika kwambili cimene tiyenela kucita kuti tipewe kuseŵenzetsa molakwika ufulu wathu , na kuti tisakhalenso akapolo a zilakolako zathu kapena a zolinga zakuthupi ? Kodi Yehova anam’patsa malangizo anji Mose ? Nanga iye anacita ciani ? Kucita zimenezo kuli ngati kutapa madzi m’citsime . ( Esitere 9 : 30 ) Pamene Yesu anali padziko lapansi , Ayuda ena anali kukhala ku Iguputo ndi madela ena a kumpoto kwa Africa , ngakhalenso ku Greece , Asia Minor ndi Mesopotamiya . M’dzikoli , nthawi zambili anthu ofatsa ndi oleza mtima amaonedwa kuti ni amantha . Iwo pamodzi na Yesu adzapanga Boma la Mulungu limene lidzalamulila anthu padziko lonse lapansi na kuwadalitsa . Kodi nimacita zonse zimene ningathe pa nchito yolalikila na kuphunzitsa anthu uthenga wabwino wa Ufumu ? Malemba amatiuza kuti : “ Moyo wanu ukhale wosakonda ndalama , koma mukhale okhutila ndi zimene muli nazo pa nthawiyo . Ngati mulalikila anthu othaŵa kwawo , mufunika kukhala “ ocenjela . ” ( Mat . Kucita zimenezi kunali kovuta , koma tinayesetsa kuwaphunzitsa cinenelo camanja kuti tizikwanitsa kukambilana nawo ndi kuwaphuzitsa coonadi . Tsiku lina pa Sondo kumasana , Kenneth na Filomena , amene akhala ku Curaçao , anapita kunyumba kwa banja lina limene amaphunzitsa Baibo . Kodi Yehova anafuna kuti Yosefe akhale m’ndende kwa moyo wake wonse ? Malamulo a Yehova amatiphunzitsa mmene tiyenela kudzisamalila ndiponso mmene tingasamalilile mabanja athu . 1 , 2 . ( a ) Timalimbikitsiwa bwanji na zitsanzo za ofalitsa amene amatumikila mokhulupilika m’magawo ouma ? Onani bokosi yakuti “ Mmene Mungalembere Bajeti ” mu Galamukani ! Nanga n’cifukwa ciani iye amayesetsa kukamba zoona nthawi zonse ? ( Tito 2 : 11 - 14 ) Tikakhala na makhalidwe abwino , anthu adzaona , ndipo ena angafike pokamba kuti : “ Anthu inu tipita nanu limodzi , cifukwa tamva kuti Mulungu ali ndi inu . ” — Zek . Ngati ndinu Mkristu amene mwatumikila kwa zaka zambili , pali zambili zimene mungacite kuti muthandize ena . Cifukwa cakuti Mboni zinali zoletsedwa m’dzikolo , tinali kusonkhana m’nyumba za abale m’tumagulu mwakabisila . ( Genesis 3 : 24 ) Baibulo silikamba kuti akerubiwo anali kudandaula kapena kuona kuti apatsidwa udindo wonyozeka . MUSADETSE THUPI LANU . Tifunika kukhulupilila Mulungu , ndipo sitiyenela kukayikila kuti iye angatithandize kupanga zosankha mwanzelu . 20 : 24 ) M’nkhani yotsatila , tidzakambilana za udindo wathu umenewu . 2 : 24 ) Cina , nchito yopanga ophunzila imabweletsa cimwemwe coculuka cifukwa imakuthandizani kudziŵa bwino Malemba okhudza zimene mumakhulupilila . Ndi zolinga za kuuzimu ziti zimene zingathandize acinyamata kukhala ndi moyo weniweni m’maganizo ? 25 : 31 - 33 ) Aramagedo idzathetsa dongosolo loipali la zinthu . 6 : 8 , 12 ; 7 : 54 - 60 ) Anthu ambili acipembedzo akhala akucita zinthu zoipa , monga kupha anthu , n’kumakamba kuti akucita cifunilo ca Mulungu , pamene m’ceni - ceni akuphwanya malamulo ake . ( Eks . 20 : 13 ) Ndithudi ! M’fanizolo , akapolo onse aŵili anaculukitsa cuma cimene mbuye wao anawasiila . Conco onse aŵili anali a khama . ( Mac 14 : 23 ) Patapita zaka , Paulo analembela Tito amene anali kuyenda naye kuti : “ Ndinakusiya ku Kerete kuti ukonze zinthu zosalongosoka ndi kuti uike akulu mumzinda uliwonse , malinga ndi malangizo amene ndinakupatsa . ” ( b ) N’cifukwa ciani tikamba kuti munthu wochedwa kuti Mphukila anacitila cithunzi Yesu Khristu ? Yehova Mulungu , kupyolela m’Mau ake Baibulo amatiphunzitsa kuona moyo ndi thupi moyenela . Ganizilani mmene Timoteyo anamvelela pamene Paulo anabwela mumzindawo . Posacedwapa aliyense wa ife adzakumana ndi zinthu zofanana ndi zimenezi . 5 : 1 - 3 . Paulo atakumbutsa Akhristu anzake za ciyembekezo cawo cokondweletsa , analemba kuti : “ Conco cititsani ziwalo za thupi lanu padziko lapansi kukhala zakufa ku dama , zinthu zodetsa , cilakolako ca kugonana , cikhumbo coipa , ndi kusilila kwa nsanje . ” ( Akol . Abwele kwa ine ! 1 : 6 ) Ndi iko komwe , munthu angakumane na vuto linalake , koma n’kukhalabe na cimwemwe mu mtima . 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani mau a pa Deuteronomo 6 : 4 ndi odziŵika kwambili ? 1 , 2 . ( a ) Kodi n’ciani cimacititsa anthu kuiwala zinthu zina zake ? Mwina mungadabwe na mmene Paulo anacenjezela Akhiristu odzozedwa za kuyofya kokhala “ mogwilizana ndi thupi . ” Anthu amakamba zinenelo zosiyanasiyana , koma limenelo si vuto kwa Yehova . PA NTHAWI ina kale , nyuzipepala ya ku Korea inali ndi mutu wa nkhani wocititsa cidwi wakuti : “ Kodi ‘ Shim Cheong Wabwino ’ Amene Sanali Kudziŵa Zilizonse za Yesu , Anapita ku Helo ? ” — The Chosun Ilbo . Akulu amene amaphunzitsa ena amathandizanso mpingo m’njila ina . Mphindi 15 sizinali nthawi yolemetsa kwa ise ndi kwa iwo . ” Conco , kaya tikumane ndi masautso ambili motani , tiyeni ticite zimene tingathe kuti tikaloŵe mu Ufumu wa Mulungu . Yehova nthawi zonse amanipatsa mphamvu , kuti nikwanitse kupilila mavuto . Nkhani iyi idzafotokoza cifukwa cake timapindula ngati tilemekeza Yehova ndi zinthu zathu za mtengo wapatali . Idzafotokozanso mmene timapindulila . PACIKUTO : Abale ndi alongo akudya cakudya ca masana pambuyo polalikila cigawo ca m’mawa ku madela a ku Siberia Nanga zimenezi zinawapangitsa kucita ciani ? Iwo angakhale oyang’anila dela , atumiki a pa Beteli , a m’Komiti ya Nthambi , a m’Bungwe Lolamulila kapena othandiza m’makomiti a Bungwe Lolamulila . Inde , n’zoona , ndipo Mwana wa Mulungu anatsimikizila mfundo imeneyi . — Ŵelengani Luka 14 : 13 , 14 . ( Yobu 37 : 14 ; 38 : 1 - 4 ) Mau a Yehova anam’khudza mtima Yobu cakuti anakamba modzicepetsa kwa Mulungu kuti : “ Ndadziŵa kuti inu mumatha kucita zinthu zonse , ndipo palibe zimene simungakwanitse . . . . ndikulapa m’fumbi ndi m’phulusa . ” — Yobu 42 : 2 , 6 . * Tsopano , tiyeni tikambilane fanizo la matalente . Caka ciliconse , makampani a fodya amaononga ndalama zambili potsatsa malonda ao kuti akope makasitomala atsopano . Ambili a makasitomala amenewa ndi akazi ndi acinyamata m’maiko osauka . Nowa anapulumuka Cigumula cifukwa ca cikhulupililo cake . Ndine wokondwa kuti zoyesa - yesa zanga zinabala zipatso . Napeza mabwenzi odalilika , amene amanithandiza kupitiliza utumiki wanga . Tinali osangalala kutumikila pakati pa anthu aubwenzi ku Nepal . Ku mayiko ena , anthu amene sakhulupilila kuti kuli Mulungu ndiponso amene amakhulupilila cisinthiko , amalimbikitsa mfundo zimene zacititsa kuti anthu asamakonde Mulungu ndi kum’khulupilila . Iyi ni nkhani yoyamba pa nkhani 9 zimene zidzafotokoza khalidwe lililonse limene mzimu woyela umabala . Mau ake amatiuza za macenjela a Satana , ndipo “ tikudziŵa bwino ziwembu zake . ” ( 2 Akor . Nkhani yoyamba pa nkhani izi idzafotokoza mmene kukonda Mulungu kumatithandizila kukhala na cimwemwe ceni - ceni kusiyana na kukonda zinthu zina zimene anthu ambili amakonda ‘ m’masiku otsiliza ’ ano . Kodi ndi njila zina ziti zimene tingaonetsele kuti timakonda anzathu ? Ndipo zimenezi zapangitsa kuti anthu ambili m’maiko ena , azikhala ndi thanzi labwino komanso moyo wautali . Anthu amasiyana ndi nyama m’njila ziŵili zazikulu . Koma niona kuti panalibe cifukwa cocitila manyazi . Zinali ngati kuti iye anali kuona mbadwa zake zikusangalala ndi madalitso amene Yehova analonjeza . ( Aheb . Ngati mukhala odzicepetsa ndi kuyesetsa kukhazikitsa mtendele , mudzadalitsidwa ngako Anthu ambili amakhala na nkhawa cifukwa cosoŵa nchito . Pa ubale umene Yosefe anali nawo na Yehova , tipezapo phunzilo lina lofunika kwambili . Ndipo palinso njila zambili za mmene tingaonetsele kuti timakonda anzathu . Kudalila Mau a Mulungu . Inoki sachulidwa kaŵili - kaŵili m’Baibo . ( 4 ) Kudalila Mulungu tikapeza anthu otsutsa . Munadziŵanso kuti tonsefe tinabadwa ocimwa cifukwa ca kusamvela kwa Adamu . Suyenela kuopa ciliconse . ” — Mat . KUKOKA FODYA KUMAVULAZA ENA Anthu ena amaganiza kuti kukanakhala kuti anthufe tinalibe udindo wopanga zosankha , sembe umoyo ni wokondweletsa kwambili . 30 “ Munthu Amene Sadziŵa Zinthu Amakhulupilila Mau Alionse ” Iye sanayambe kulamulila nthawi imeneyo atapanga pangano la Ufumu ndi ophunzila ake . Si mafumu onse anali kutsatila malangizo a Mulungu polamulila anthu Ake akale . Udindo waukulu umabwelanso na ulamulilo waukulu . Mpamene munthu amaonekela kuti ni wodzicepetsa kapena ayi . Coyamba , angaphunzile kuti mfundo za m’Baibulo zimalimbikitsa mgwilizano ndi umodzi . “ Atate wanu amadziŵa zimene mukufuna musanapemphe n’komwe . ” — Mateyu 6 : 8 . Nkhani ziŵilizi zikuyankha mafunso amenewa . Ngati tidalila Yehova ndi ziphunzitso zake , tidzakhala aphunzitsi abwino . Ndipo zimenezi zidzapindulitsa ifeyo ndi onse otimvela . ( 1 Tim . Mkupita kwa nthawi , ine ndi mkazi wanga tinabatizika n’kukhala Mboni za Yehova . Lusitara unali mzinda waung’ono umene unali kudela la kumidzi m’cigwa cokhala ndi madzi ambili . “ Cifukwa ca Mau ake , Baibulo , n’naleka kukhala wokhumudwa . Koma nthawi zina , thandizo linali kucokela kumene sitinali kuyembekezela . ( a ) N’cifukwa ciani nthawi zina zingakhale zovuta kuthandiza ofooka ? Ngati mumaona kuti kucita ulaliki wapoyela n’kovuta , musabwelele m’mbuyo . Pa cifukwa cosadziŵika bwino , io anali kukhulupilila kuti munthu wodwala amacila mozizwitsa akalowa m’dziwelo pamene madzi akuwinduka . Kodi kutumikila ku malo kumene kukufunika anchito ambili kwamukhudza bwanji Hiroo ? 10 - 12 . ( a ) N’kuthenga kuti Satana anacita ciani poseŵenzetsa nyambo imene anakopa nayo anzake ? Wosimba ni Samuel Hamilton Dzikolo linali ndi nyumba zazikulu zokongola ndipo linali lotukuka . Komanso , tiyenela kukumbukila kuti sitingadziŵe zonse zokhudza nkhaniyo . Mwacitsanzo , tingalephele kukhala oleza mtima , tingamakwiye msanga , kapena kudandaula kwambili za anthu ena . Monga mmene takambila poyamba paja , Paulo ayenela kuti anacezelanso mzinda wa Lusitara patapita zaka ziŵili kapena zitatu . Umu ni mmene mtsikana wina wa zaka 13 anakondwelela , atalandila kagalu monga mphatso . Pamene Sukulu ya Ulaliki inayamba mu 1943 , ndinayamba kukamba nkhani za m’sukulu mumpingo . Nthawi zina , kusiyana kwa zibadwa kungacititse kuti tisakhale omasuka kuceleza anthu ena . Davide anakamba kuti Yehova ndiye anamuthandiza kupha zilombo zolusa Nkhani ino idzatithandiza kupilila ndi kutilimbikitsa kuika maganizo athu pa Mulungu ndi Ufumu wake . Nkhani yoyamba idzafotokoza mavuto amene abale na alongo othaŵa kwawo amakumana nawo , na zimene ife tingacite kuti tiwathandize . Maganizo olakwika amene mwanayo anali nawo ndi nkhani yaing’ono ndiponso yoseketsa . 2 : 9 ) Koma Satana angatisoceletse mwa kugwilitsila nchito “ cinyengo camphamvu ca cuma . ” Mbali zovuta anazilemba m’mau amene timakamba tsiku lililonse . Tasindikizanso makope a Baibulo la Dziko Latsopano oposa 200 miliyoni m’zinenelo zoposa 130 . Potsilizila pake , anadalitsidwa cifukwa colimbikila . ( Num . 9 : 6 ) Komanso , zimene Yosefe anacita , zoika Yesu m’manda zikanacititsa kuti anzake asamam’lemekeze . Anthu onse amafa cifukwa cakuti munthu woyamba anakana kutsogoleledwa ndi Mlengi . — Ŵelengani Genesis 1 : 27 ; 2 : 15 - 17 . 7 : 9 ) Zozizwitsa zimenezo zinasonyezanso kuti Mwana woyamba kubadwa wa Mulungu amakonda kwambili anthu . ( Yoh . ( b ) Kodi kuganizila zimene zidzacitika mtsogolo kuyenela kukhudza bwanji mmene timaonela cuma cakuthupi ? Nthawi zina , anthu atsopano m’coonadi , amapempha ofalitsa ena okhwima mwauzimu kuti awathandize kuphunzitsa ana awo coonadi , mwina ngakhale kuwaphunzitsa Baibo . ( Aef . 2 : 3 ) Mwacitsanzo , ngakhale kuti timalandila malangizo mobweleza - bweleza pa nkhani ya kavalidwe , ena akupitilizabe kuvala mosadzilemekeza komanso kudzikonza mosayenela . Kodi buku la m’Baibulo limeneli linalembedwa bwanji ? André ndi Gabriela anavomeleza kuti : “ Zimenezi zinatipatsa mwai wina wotumikila Yehova , ndi kuika pambali zofuna zathu . ( a ) Fotokozani khalidwe la anthu ambili masiku ano . ( b ) M’mbili yonse ya anthu , ndani amene Mulungu wathandiza ? ( Mateyu 7 : 12 ) Koma kodi cipembedzo coona cimangolimbikitsa makhalidwe abwino ? Kodi kudziŵa kuti Baibulo inasinthidwa kapena ayi kuli ndi phindu ? Masiku anonso , Yehova amamvetsela malonjezo amene timapanga . NYIMBO : 84 , 73 Conco mukakhala ndi nkhawa , mwacifundo iye ‘ angakuthandizeni ’ ‘ pa nthawi imene mufunika thandizo . ’ Umu ndi mmene maulosi ambili analembedwela pambuyo pake . 4 : 13 ) Kuganizila mayankho athu pa mafunso amenewa kungatithandize kudziŵa mmene tapitila patsogolo mwauzimu . Mosapita m’mbali anauza omvetsela ake kuti : “ Lekani kudziunjikila cuma padziko lapansi . . . . ( 3 ) Kugwilitsila nchito cinenelo cosavuta kuŵelenga ndi kumva . Cilamulo ca Mulungu cinalinso ndi mfundo zina zimene zinali kuthandizanso oweluza kugamula milandu mwacilungamo , ngakhale pa milandu yovuta kwambili . Mungaŵelenge nkhani ya Yosefe yocititsa cidwi m’buku ya Genesis , macaputa 39 mpaka 41 . Anatinso : “ Ninapempha Yehova kuti anithandize kukonda anthu a m’gawo langa . Kodi cilengedwe cimatiphunzitsa ciani ponena za Yehova ? Ndipo ulendowu uyenela kuti unali wotopetsa . ” Komanso , ena sanali kukwanitsa kuŵelenga khadi lathu . Kucita izi kudzalimbitsa mipingo yonse padziko lapansi ndi kuthandiza aliyense wa ife kukhala okhulupilika makamaka pa nthawi yapadela imene ikubwela . Ngati makolo apitiliza kuphunzitsa ana awo moleza mtima , pang’ono ndi pang’ono anawo adzadziŵa “ m’lifupi ndi m’litali ndi kukwela ndi kuzama , ” kwa coonadi . ( Aef . TSAMBA 8 • NYIMBO : 119 , 17 Mngelo uja anafotokoza kuti mkaziyo dzina lake ni “ Kuipa . ” 43 : 10 . N’cifukwa ciani mafanizo ni othandiza ? Nanga mayi wina anaonetsa bwanji zimenezi ? Paulo anali kukumbukila kuti kale anali “ wonyoza Mulungu , wozunza anthu ake ndiponso wacipongwe . ” Koma kuti akhale na cimwemwe ceni - ceni afunika kukhala pa ubwenzi na Yehova , amene amachedwa “ Mulungu wacimwemwe . ” ( 1 Tim . Komabe , Mulungu anasankha anthu ocepa kuti adzakhale kumwamba ndipo adzapatsidwa matupi auzimu . ( Aheberi 10 : 24 , 25 ) Tifunika kukonda kwambili abale athu tsopano , cifukwa cikondi cimeneci cidzatithandiza kupilila ziyeso zilizonse zimene tingakumane nazo mtsogolo . 3 , 4 . ( a ) Kodi Yesu anapeleka fanizo lotani poyankha funso lakuti : “ Nanga mnzanga amene ndikuyenela kumukonda ndani kwenikweni ” ? M’caka ca 1972 , udindo woyang’anila mpingo unapatsidwa ku bungwe la akulu m’malo mwa m’bale mmodzi woyang’anila mpingo . Conco , timafuna kuti iwo aone kuti sitifuna kuphonya msonkhano umenewu , kupatulapo ngati pali vuto lalikulu kwambili . N’zoona kuti si nthawi zonse pamene tingalankhule kapena kucita zinthu zimene Yehova afuna kuti ticite . ( b ) Tikambilana mafunso ati m’nkhani ino ? Tingaike motani maganizo athu pa zinthu zakumwamba ? Polankhula ndi Mulungu Wamphamvuyonse , Yobu anadziyankhila funso lake kuti : “ Inu mudzaitana ndipo ine ndidzayankha . Iwo anandiuza kuti ndiŵelenge malemba m’Baibulo langa la King James Version . Ni mapindu ena ati amene timapeza tikakhala owoloŵa manja ? Iye amafuna kuti makolo aphunzitse ana ao kuti ayambe kum’tumikila . Kuŵelenga mau a Yehova m’Baibulo lokonzedwanso la 2013 , kuli ngati kutenga cinthu camtengo wapatali m’thumbalo ndi kuyang’anitsitsa kukongola kwa cinthuco . Kaya mudzalandila madalitso amenewa kapena ai , zidzadalila inu . Conco , tifunika kukhala pa mtendele na Akhristu onse ndiponso kukhala nawo pa ubwenzi wolimba . Ungalembe chati na kuikapo malemba oonetsa mmene Mulungu anaunikila pang’ono - pang’ono zokhudza anthu na makonzedwe ochulidwa pa lemba limeneli , na mmene ulosi umenewu udzakwanilitsidwila . Popeza anthu ambili amaona kuti kugwila nchito yapamwamba ndiye cinthu cofunika ngako , n’zosavuta Mkhristu kutengela maganizo aconco . Kwa zaka zoposa ziŵili , tinakhala ndi mwai woyendela maiko osiyanasiyana kukaphunzitsa magulu a omasulila . Tingathandize m’bale kapena mlongo wacikulile amene amavutika kuyenda popita kumisonkhano . Kodi Yehova amaiona bwanji nchito ? Ndipo amacita ciani ? Mwacitsanzo , ku Asia , kamtsikana ka zaka zisanu , makolo , ndi agogo ake anali kukonza seŵelo lonena za ulendo waumishonale wa mtumwi Paulo m’cipinda cocezela . Nanga ndani ameneyu ? ” Kuganizila vesi limeneli kudzatithandiza kuyamikila kwambili Yehova cifukwa ca cikondi ndi cisamalilo cimene amationetsa . Ndi madalitso otani amene munthu angapeze cifukwa codzipeleka ? Mu 1923 , kodi anthu a Mulungu analimvetsa bwanji fanizoli ? Makolo ayenela kuphunzitsa ana ao kuti asamaseŵele kapena kuthamangathamanga m’Nyumba ya Ufumu . — Mlal . Cinthu coyamba cimene tingacite ndi kutsatila ndandanda ya kuŵelenga Baibulo pa nyengo ya Cikumbutso . 3 : 16 ) Mwina tsopano ndinu wotsimikiza mtima kwambili kukhalabe woyela , osati cabe cifukwa cakuti n’zimene Yehova amafuna , koma cifukwa cakuti timafunikila kucita zinthu zom’kondweletsa . Ena amapewa zosangulutsa zimene sizolakwika koma zimene zingawacititse kukhala ndi zilakolako zoipa . ( Sal . Tsopano ndakhala muutumiki wa nthawi zonse kwa zaka 10 . 10 : 38 ) Ndiponso , mzimu woyela unathandiza Yesu kukhala ndi makhalidwe abwino , monga cikondi , cimwemwe , ndi cikhulupililo colimba . ( Yoh . 15 : 9 ; Aheb . ( Aroma 8 : 38 , 39 ) Tiyembekezela mwacidwi kudzaonana naye m’dziko latsopano la Mulungu akadzaukitsidwa . — Yoh . 5 : 28 , 29 . Ophunzila a Yesu oyambilila anali kukamba Ciheberi , koma iye atamwalila , ophunzilawo anayamba kukambanso zinenelo zina . Yesu anadalitsidwa kwambili cifukwa cakuti anakhala womvela mpaka imfa . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kulimba mtima patsiku lomaliza la moyo wake padziko lapansi ? ( 1 Mbiri 17 : 1 - 4 , 11 , 12 ; 22 : 5 - 11 ) Nayenso Brook anati : “ Yehova anafuna kuti tigogode pa citseko cina . ” Tsopano gulu lathu lakula , cakuti ciŵelengelo ca ofalitsa cipitilila 5,000 . Ndipo amayamikila Yehova cifukwa com’thandiza kukhala wofatsa . ( Luka 2 : ​ 41 , 42 ; Machitidwe 2 : ​ 1 , 5 - 11 ) Conco , alendo onse amene anali kufika pa zikondwelelo zimenezi anali kufunika kupeza malo ogona . Iye sanalephele kulandila azondiwo cifukwa coopa mfumu ya Yeriko ndi anthu ake . N’cifukwa ciani tiyenela kutsatila malangizo a pa 1 Akorinto 10 : 32 , 33 pa nkhani ya mavalidwe ? ( b ) tingawalimbikitse bwanji ? Ngati nanunso mumaona conco , Yehova angakuthandizeni kukhala wolimba mtima . Mwanzelu , muthandizeni kulimbitsanso cikhulupililo cake . Ngakhale kuti kukamba nkhani sikunali kopepuka , ana naonso anali kukamba nkhani m’sukulu . 11 : 3 - 12 ) , 11 / 15 ( a ) N’ciani cingacitike ngati makolo atumizila cabe ana mphatso m’malo mokhala nao ? Nanga zinthu zili bwanji masiku ano ku Cuba ? Conco , uziseŵenzetsanso mutu kuti upeze cidziŵitso colongosoka . Tidzaonanso mmene tingapewele kucita colakwa ngati cimene Mose anacita . Ngakhale kuti mwina anali ndi zaka za m’ma 60 , anakwanitsa kuyenda m’madela acilendo , na kukhala umoyo wovutitsa . Analibe ciyembekezo cakuti angabwelelenso kwawo . Koma m’kupita kwa nthawi anayamba kuona kuti zisangalalo za m’dzikoli sizinali zokhutilitsa ndipo ndi zopanda phindu . Tinali kufunitsitsa kupeza boti loyendela mphepo kuti tilisandutse kukhala boti la injini lakuti tizikhalamo . Maluŵawo afota . Koma mawu a Mulungu wathu adzakhala mpaka kalekale . ” — Yesaya 40 : 8 . Kuciyambi , kuli mlongoza nkhani amene angatithandize m’njila zosiyana - siyana . Tiyelekezele kuti mkazi wokwatiwa akugula zinthu m’sitolo , kenako waona nsapato zabwino kwambili . vesi 13 Kwa zaka zambili , okana Kristu acititsa anthu mamiliyoni ambili kukhala mumdima wa kuuzimu . Mwina timayesetsa kupewa zinthu zimene Mulungu amazonda . Palibe munthu amene ali na ulamulilo waukulu kupambana Mulungu . Kodi nchito yolalikila imatipatsa mwayi wotani ? 17 : 17 ) Koma Solomo sanamvele lamulo limeneli cakuti m’kupita kwa nthawi anakwatila akazi 700 . Pa zimene takambilanazi , ngati pali zinthu zina zimene mufunika kusintha kuti mupewe zilakolako zoipa , muyenela kucita zimenezo mwamsanga . 22 : 6 ) Monga amatiuzila Malemba , mayiyu anam’tulila Yehova nkhaniyo m’pemphelo . ( Sal . Yehova anasintha maganizo ake pamene zinthu zinasintha . ( 1 Maf . N’cifukwa ciani kuganizila mosamala zimene Mose anacita n’kofunika ? Makolo ambili amacita bwino pa nkhani imeneyi . Tikamasinkha - sinkha za cilengedwe ca Yehova , timakumbukila kuti iye ndi wacikondi , wanzelu ndiponso wamphamvu . ( Sal . Tinaganiza zoyamba upainiya . Poyamba Choong Keon anaona kuti sanali kucita zambili mumpingo cifukwa cosadziŵa bwinobwino Cichaina . Komanso sanakambe zinthu zimene zikanakhumudwitsa ena . Nzelu yeni - yeni imaoneka mukaiseŵenzetsa . Woyang’anila nchito wina anati ciani ponena za tumapepala twauthenga ? Cifukwa cakuti macaputala a m’Mabaibulo ao anali atagaŵidwa mosiyanasiyana . Liuli lingamasulidwe monga mlowam’malo . Mwacitsanzo , lingamasulidwe kuti “ amene ” kapena “ iwo . ” Kugonjetsa Imfa “ Iye adzameza imfa kwamuyaya ndipo Yehova , Ambuye Wamkulu Koposa , adzapukuta misozi pankhope zonse za anthu . ” — Yesaya 25 : 8 . Koma kodi tingaonetse bwanji kuwala kwathu m’mbali zitatu zimenezi ? — Ŵelengani Mateyu 5 : 14 - 16 . Ndipo Davide anali munthu weni - weni . Nkhanizi zidzafotokoza . Kodi mungakambilane bwanji za Baibulo ndi anthu ? Ndipo colinga canu ciyenela kukhala ciani ? Tikamaika nchito yolalikila patsogolo , kodi timaonetsa bwanji kuti timakhulupilila Yehova ? A Willie anali mmodzi wa Mboni za Yehova , ndipo apa m’pamene amayi anayambila kumva coonadi ca m’Baibo . Nyumba za Ufumu zoposa 100 ndi nyumba za Mboni za Yehova zoposa 1,000 zinaonongedwa panthawiyo . Ndi zinthu zina ziti zimene zatithandiza pa nchito yathu yolalikila padziko lonse ? Iye anatumizidwa kuti akathandize kumanga Nyumba ya Ufumu ndi nyumba ya amishonale pacilumba ca pa Nyanja ya Pacific . 6 : 10 ; Luka 11 : 2 ) Kuti awakhazike mtima pansi , Yesu anafotokoza mmene Yehova amasamalila zolengedwa zake . Patapita nthawi yocepa kucokela pamene tinakwatilana , ine ndi mkazi wanga tinathawila ku Austria . Kodi Yehova watithandiza bwanji kumvetsa fanizo la nkhosa ndi mbuzi ? 12 : 6 ) Zimene anakambazo zinanikhudza mtima na kunithandiza kuyambanso kutumikila Yehova mwacimwemwe . Timapindula bwanji ndi imfa ya Yesu ? Mwana wina angakhale ndi luso locita maseŵela ena ake pamene wina angakhale ndi luso lojambula zithunzi ndi manja kapena lopangapanga zinthu . ( Maliko 15 : 1 , 43 ) Conco Yosefe anali mmodzi wa atsogoleli a Ayuda . N’cifukwa cake anali na ufulu wokaonana ndi bwanamkubwa waciroma . MAKHALIDWE A ANTHU : Baibulo limati “ masiku otsiliza , ” adzadziŵika ndi kuloŵa pansi kwa makhalidwe abwino . Kodi munthu amene amacitila ena cifundo amapindula bwanji ? Tinakambilanso za anthu abwino amene tingaziceza nao . Ena amene kale anali oyang’anila anatsitsidwa pa maudindo . Ndipo zimenezo zinawacititsa kudziona monga analephela udindo wao . Mwacitsanzo , panthawi ya ulamulilo wopondeleza wa Nazi ndi wa cikomyunizimu , Yehova anathandiza akazi okhulupilika kukhalabe okhulupilika kwa iye . MTUMWI Paulo ayenela kuti analemba kalata yake yopita kwa Akhristu a ku Kolose ca pakati pa 60 C.E . na 61 C.E . ( b ) Kodi tidzakambilana zitsanzo za anthu ati auzimu ? Matica a pa sukuluyo sanakondwele , ndipo ananiwopseza ndi kuninyengelela kuti nisinthe maganizo anga . Kodi lemba la Salimo 118 lionetsa bwanji kuti ulosi wakuti akufa adzauka ungakwanilitsidwe ngakhale pambuyo pa zaka zambili ? 17 : 10 , 11 ) Malinga ndi pangano limeneli , Abulahamu ndi amuna onse a m’banja lake anadulidwa . Ŵelengani Nyimbo ya Solomo 8 : 6 . Conco , nyumbayi si ya munthu kapena ya mpingo mosasamala kanthu za dzina limene lili pa mapepala a kuboma . Kugwila nchito kwambili sikunasinthe ciliconse . N’cifukwa ciani kupanga zosankha mwanzelu n’kofunika kwambili ? Tiyeni tiŵelenge mavesi 22 , 23 , ndi 28 . N’cifukwa ciani tingakambe kuti pamene Mose anamenya thanthwe , mwina anacititsa Aisiraeli kukayikila kuti Yehova wacita cozizwitsa ? Lamekiyo atabadwa , Inoki , amene anali ambuye ake , anaptilizabe kukhala na moyo kwa zaka zoposa 100 . Ŵelengani 1 Akorinto 15 : 33 . Enanso amaika zinthu zimenezi pa katundu wogulitsa , kapena pa mapulogilamu a pa zipangizo zamakono . Tsiku lililonse akadzuka m’maŵa , mwina Yosefe anali kuyembekezela kuti atuluka m’ndendemo . Koma masiku anali kungopita , zinthu osasintha . ( Mateyu 24 : 3 , 7 ; Luka 21 : 10 , 11 ) Iye anauza ophunzila ake kuti mavuto amenewa adzapanga cizindikilo ca masiku otsiliza . Ngakhale kuti makolo anga ananipitikitsa pa nyumba pawo , Yehova wanipatsa banja lalikulu la okhulupilila anzanga . Conco , io akucita mantha kwambili kuti mwina tikufika m’nthawi imene zocita za anthu zikuonongelatu dzikoli , ndipo amakamba kuti zimenezi zingapangitse nyengo kusintha mwadzidzidzi ndi kucititsa mavuto oopsa . Conco , n’naleka kugwilizana ndi anzanga oipawo , ndipo n’napeza mabwenzi mumpingo woona wacikhiristu . Anthu amenewa amathetsa kusamvana pogwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo osati ndewo . Nzelu yaumulungu ni imene inam’thandiza kudziŵa kuti ayenela kugonjela olamulila a dziko kupatulapo ngati apeleka lamulo losemphana na malamulo a Mulungu . Ndipo tidziŵa kuti ena akukumana ndi mavuto ambili pa nthawi imodzi . Ndipo onetsani kuti mumawakonda . Paulo analimbikitsa Timoteyo kuti : “ Pitiliza kukhala wodzipeleka poŵelenga pamaso pa anthu , powadandaulila , ndi powaphunzitsa . Nanga bwanji inu ? Kodi mumaonetsa cifundo kwa odwala na okalamba mwa kuyesetsa kuwathandiza pa mavuto awo ? — Afil . ( b ) Nanga mungacite ciani kuti muzithandiza oyang’anila dela ? Coonadi cimeneci cipezeka m’Baibulo . Palibe amene amafika kwa Atate osadzela mwa ine . ’ ” 1 : 6 . 8 Muzilemekeza Amene Afunika Kulandila Ulemu Ndiponso timakhala okonzeka kukhululukila ena monga mmene Yehova amacitila kwa ife Zindikilani zimene eninyumba amakonda , ndipo sankhani mau anu moyenelela ( Onani ndime 15 ) Mmene timacitila zinthu ndi ena zimaonetsa ngati timatsanzila cikondi ca Mulungu kapena ayi . Nditamvetsela vuto lao , ndinawauza mmene Yehova anandithandizila kulimbana ndi vuto lofananako . ( Num . Tsiku lina pamene ndinali kukhala m’galimoto yanga , ndinafika pa Nyumba ya Ufumu kukali maola angapo kuti msonkhano wokonzekela ulaliki uyambe . 30 : 8 ) Kuyambila m’nthawi zakale , atumiki a Yehova anali kupita ku madela ena kukafunafuna cakudya . Mu Ulamulilo wa Kristu wa Zaka 1000 , mwina zidzatenga nthawi kuti olungama ndi osalungama akhale angwilo . ( Mac . Ndiye Suntuke anaganiza kuti : ‘ Zoona Eodiya sananiitaneko ine ! N’nakonzanso msonkhano wa cigawo m’bwalo ina yochuka ya maseŵela mumzinda wa Manaus . Kodi tili na mipata iti ‘ yoceleza ’ ena ? 1 , 2 . ( a ) Kodi anthu amaganiza bwanji pa mfundo yakuti Mulungu ali na gulu ? 12 : 11 ) Cacitatu , akulu anapatsiwa udindo wolimbikitsa wolakwa amene walapa , ndipo anaphunzitsidwa mocitila zimenezi . Amayi anapitiliza kuphunzila Baibulo mwakabisila , ndipo anayamba kukonda zimene anali kuphunzila . Mtendele wa mumtima unatithandiza kukhala na mphamvu zofotokozela atolankhani za ciyembekezo cathu ca ciukililo . M’bale waciŵili anati : “ Malemba monga 2 Akorinto 10 : 5 , lonena za ‘ kumvela Kristu , ’ andithandiza kukhala womvela ndi kugwilizana ndi amene akutsogolela . Kukhala wacifundo kudzatisonkhezela kuthandiza anthu makamaka amene ali ngati bango lophwanyika , kapena cingwe ca nyale comwe catsala pang’ono kuzima . Tisakhale monga atsogoleli acipembedzo a m’nthawi ya Yesu . ( Mat . ( 1937 ) , Nov . “ Pamene iye anali kuzengeleza , [ angelo ] , mwa cifundo ca Yehova pa iye , anagwila dzanja iyeyo , mkazi wake , ndi ana ake aakazi aŵiliwo , n’kuwatulutsa kukawasiya kunja kwa mzinda . ” N’cifukwa ciani zilakolako zoipa zingatimanitse mphoto ? ( Ŵelengani Luka 1 : 26 - 33 . ) Fotokozani mwacidule nkhani imene ili m’Nyimbo ya Solomo . Kudalila Mulungu kunamuthandiza kucita zinthu zambili zabwino . Ndipo pambuyo pake , mwanayo wapatulako ndalamayo n’kupatsa makolowo monga mphatso . Zaka pafupifupi 4000 zapitazo , Sara , mkazi wa Abulahamu anali kukhala kumwela kwa Betelehemu . Mwadzidzidzi , iye analandila alendo atatu ndipo anawaphikila “ mkate ” umenewu . Monga Akristu , tiyenela kucita zinthu moona mtima ndi anthu onse kuphatikizapo anchito athu . 1 : 5 , 16 . Ndipo mwa apa ndi apo , ndinali kugwila nchito ndi gulu la zigaŵenga . Kodi Mboni za Yehova Ndi Anthu Otani ? Komabe , n’zomvetsa cisoni kuti timafa . Iwo anali a Mboni za Yehova , ndipo anandipatsa buku lija limene wansembe analetsa . Magazi amene Yesu anakhetsa ndiwo umboni wa pangano latsopano . Mwacitsanzo , pamene Aisiraeli anali m’cipululu ca Sinai , Yehova anawalamula kuti amange malo olambilila . Iye anapilila mavuto aakulu oika moyo wake paciopsezo na zoipa zina zimene anthu ena anam’citila . Mosakaikila , mungaculenso mkazi kapena mwamuna wanu ndiponso ana anu . Dzina la Mulungu m’cidutswa ca mpukutu wa Septuagint wa m’nthawi ya Yesu Zimenezo zinali zoona ! Koma Sara anakhalabe wokhulupilika kwa Mulungu ndi kwa mwamuna wake . Takhala tikupemphanso kuti mukhale odziŵa molondola cifunilo cake [ Mulungu ] , ndiponso kuti mukhale ndi nzelu zonse komanso muzimvetsetsa zinthu zauzimu . Koma Davide atadziŵa zeni - zeni zokhudza Mefibosetiyo , anasintha maganizo ake . ( 2 Sam . ( Akol . 1 : 11 , 12 ) Koma ngati tiyembekezela modandaula cifukwa coona monga kuti Yehova sakucitapo kanthu mwamsanga , tikhoza kum’khumudwitsa . — Akol . 25 : 40 . Mkulu wa asilikaliyo anakhala cete kwa nthawi yaitali kuganizila za nkhaniyi . Anakhazikitsa kumwamba mozindikila . ” ( Miy . Kulephela kudya na kumwa . Lemba la Miyambo 24 : 10 limati : “ Ukafooka pa tsiku la masautso , mphamvu zako zidzakhala zocepa . ” Pa Pentekosite mu 33 C.E . , Ayuda ambili pamodzi na ŵanthu otembenukila ku Ciyuda anadzozedwa na mzimu woyela . Anati : “ Timathandiza ana athu kuti azilemekeza moyo ndi kudziŵa kuti ni wodabwitsa kwambili . ” ( Ŵelengani Chivumbulutso 18 : 4 . ) N’cifukwa ciani sitiyenela kumuyopa maningi Mdyelekezi ? Izi zitsimikizila mfundo yakuti “ kunyada kumafikitsa munthu ku ciwonongeko , ndipo mtima wodzikuza umacititsa munthu kupunthwa . ” Kodi simunakondwele kuti munatonthoza wina wake tsikulo ? Pamenepa tikupezapo njila ina imene tingaonetsele kuti timamuyamikila Yehova potisankha kukhala anthu ake . Pambuyo pake , makalata oyamikila anaikidwa m’magazini a mwezi umenewo . Pa Levitiko 10 : 1 - 11 , timaŵelengapo cocitika cimene cinabweletsa cisoni ku banja la Aroni . Popeza kuti Yehova ndi Mulungu wacikondi , iye sakondwela ndi zoipa . Koma iye anali kucenjeza otsatila ake odzozedwa kuti afunika kupitiliza kucita khama kapena ‘ kucita malonda ndi matalente ao ’ ndi kupewa kukhala monga kapolo woipa . — Mat . N’zosacita kufunsa . Ngati mwana wanu akaikila ciphunzitso cina cake , osayankha mokhumudwa . Zocita zathu ziyenela kusonyeza kuti timakhulupililadi Mulungu ndi Yesu . Kodi kudzipatulila na kubatizika kwathu kumaonetsa ciani ? Paulo anali kudziŵa kuti sanafunike kuonetsedwa cifundo cacikulu ca Mulungu cifukwa anali kuzunza Akhiristu . ( Yakobo 1 : 3 ) Mabwenzi oipa amaononga cikhulupililo , koma mabwenzi abwino amacilimbitsa . Kucita izi kudzatithandiza kupeza mfundo za coonadi zimene zingakhale zatsopano kwa ife . ( Yos . NKHANI ZOPHUNZILA Tikacita cinthu cabwino , timakondwela anthu akatiyamikila ndipo timaona kuti n’zoyenelela . Ganizilani zimene iye anauza mneneli Ezekieli zokhudza kugwilizanitsa ndodo “ ya Yuda ” ndi “ ya Yosefe ” kuti zikhale ndodo imodzi . Nyumba ya Ufumu yatsopano ikangomangidwa , tiyenela kumaiyeletsa nthawi zonse kuti izipeleka cithunzi cabwino ca Mulungu amene timalambila yemwe ndi wadongosolo . Kukonda Mulungu kumatithandiza kupewa kalikonse kamene kamadetsa thupi . Zacitikapo kuti eninyumba amene poyamba anali aukali asintha khalidwe lao cifukwa anthu a Yehova anawayankha mofatsa ndi mwaulemu . — Miy . Citsanzo ca Yosefe ciyenela kuti cinam’thandiza kwambili Yefita . Kodi atumiki okhulupilika a Yehova akale anali kucilikiza bwanji nchito yake ? 3 : 5 , 6 . N’cifukwa Ciani Tiyenela ‘ Kukhalabe Maso ’ ? Ophunzila Baibo anga ena , lomba ni apainiya ndi akulu mumpingo . Koma monga mkaidi , iye anali kukhala movutika ndithu . Timatonthozedwa ndi Mulungu “ Atamandike Mulungu ndi Atate wa Ambuye wathu Yesu Kristu , Tate wacifundo cacikulu ndi Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , amenenso amatitonthoza m’masautso athu onse . ” — 2 Akorinto 1 : 3 , 4 . Iye sanacite zinthu mofanana ndi mmene Sauli ndi asilikali ake anacitila . Ngati munthuyo ayankha kuti iyai , tingam’funse cifukwa cake anayamba kukaikila ngati Mulungu aliko . M’bale wathuyu ndiponso bwenzi lathu , anasiya mkazi , ana 6 , adzukulu ndi adzukulutudzi . ( Mat . 10 : 34 - 37 ) Anthu amenewa akakufooketsani , mungayambe kuganiza kuti kudzipeleka kwanu ndi kopanda phindu ndi kuti simungakwanilitse utumiki wanu . Koma pambuyo polalikila pamodzi na Mboni zaciyela ndi kukaceza kunyumba zawo , mlongoyu anati : “ Iwo ni anthu monga ife . ” Tidziŵa bwanji kuti Mose anaika maganizo ake pa kucita cifunilo ca Mulungu ? Patapita zaka 16 , nchito yomanga kacisi wa Yehova inaimilatu . Kodi amacita ciani kuti acepetse vuto limeneli ? Koma inu musasoceletsedwe . Conco , muyenela kutumikila Yehova mwa kufuna kwanu osati cabe cifukwa cotengela makolo anu kapena munthu wina . ( a ) Ndi phunzilo lanji lokhudza kuloŵa m’banja limene tingatengepo pa nkhani ya Yehosafati ? Kodi kum’dziwa bwino Yehova kunawathandiza bwanji kuti akhalebe na mtima wosagawanika ? Pambuyo pake , abale athu anayi nawonso anakhala Mboni zokhulupilika . Kodi Yesu anawalimbikitsa bwanji ? Davide analemba kuti : “ Ndidziŵitseni njila zanu , inu Yehova . 13 : 35 ; Yak . 2 : 8 ) Ndipo njila yaikulu imene timaonetsela kuti timakonda Mulungu , Kristu , ndi anzathu , ndi mwa kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu . — Yoh . 15 : 10 ; Mac . 1 : 8 . ( 2 Samueli 7 : 22 ) Cotelo , mau a Mose anali kukumbutsa Aisiraeli kuti afunika kulambila Yehova yekha . Conco , n’naganiza zoyamba kutumikila mwakhama kuti nipeze cuma cauzimu . ” Komabe , kukhala ndi nkhawa kwambili kumayambitsa matenda ndipo kungaticititse kusiya kukhulupilila Yehova . ( Yes . 60 : 22 ) Ulosi umenewu ukukwanilitsika m’masiku ano otsiliza . Kenako kunayamba kuda . M’kupita kwa nthawi , dziko lapansi likanadzala na ŵanthu pamlingo woyenelela , ndipo akanafutukula paradaiso kufika kumalekezelo a dziko lapansi . Yesu adzabwela kudzaononga dzikoli . Conco , tifunika kukonzekela . Kukoma mtima kwa Boazi kunaonetsa cisomo ca Yehova kwa mtsikana amene anathaŵila “ m’mapiko mwa Mulungu wa Israeli kuti apeze citetezo . ” ( Rute 2 : 12 , 20 ; Miy . 28 : 10 ) Komabe , n’zacisoni kuti nthawi zambili Aisiraeli sanali okhulupilika . Iye amaona kuti tonse ndife ofanana . ( a ) N’ciani cimene ciyenela kulimbikitsa akulu kuphunzitsa ena ? Mwacitsanzo , ngati tifuna kuyamba utumiki wa nthawi zonse , tingadzifunse kuti , N’ciani cidzacitika nikadzadwala ? N’ciani cingatipangitse kusintha cosankha cimene tinapanga ? M’zaka zaposacedwa , m’gululi mwakhala mukucitika nchito zambili zocititsa cidwi . N’napatsidwanso mwayi wotumikila monga mkulu mu mpingo wa Fulham . N’zothekanso kutumiza mwekha zopeleka zanu ku ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova m’dziko limene mukhala . Tinaitaniwa kuti tikatumikile pa ofesi ya nthambi mu United States . Apa n’kuti papita zaka 38 kucokela nthawi yoyamba pamene tinafunsila utumikiwu . Kodi mudzalimba mtima ndi kuwafotokozela mosamala cifukwa cake mumawaletsa ? ( Gen . 26 : 34 , 35 ) Iye anali wosiyana ngako na Yakobo , amene anaonetsetsa kuti wakwatila mkazi wolambila Mulungu woona . — Gen . Sitikudziŵa . Zocita zawo zimaonetsa kuti ubwenzi wawo ndi wozikidwa pa cikondi osati pa udindo kapena utumiki wawo . Munthu akabatizidwa , amakhala ndi mwai wolandila madalitso ambili ocokela kwa Yehova , koma m’pamenenso Satana amayamba kum’tsutsa kwambili . Kumbukilani kuti Yesu anatiphunzitsa kupemphela kuti : “ Ufumu wanu ubwele . Pamene tiŵelenga Baibulo ndi zofalitsa zathu , tiyenela kusinkhasinkha zimene tikuphunzila ndi kuona mmene tingapindulile ( Salimo 51 : 5 ; Yohane 8 : 34 ) Olo tiyesetse bwanji , patekha sitingadzimasule ku ukapolo umenewo . Conco mwa kupeleka moyo wake monga nsembe , Yesu anaombola anthu ku ukapolo wa ucimo . Satana Mdyelekezi atacotsa Adamu ndi Hava kwa Mulungu , anapitilizabe kusoceletsa mtundu wa anthu mpaka lelo . — Yoh . Zofalitsa zodzala masaka aŵili zinali kutha mwezi umodzi cabe . Yosefe anali wao tsopano ndipo sanasiye kumuyang’anila . Seth * anakamba kuti : “ Nchito yanga ndi ya mkazi wanga inatha pa nthawi imodzi . ( 1 Sam . 15 : 3 , 9 , 15 ) Yehova ni Woweluza wacilungamo . Iye amadziŵa za mumtima mwa munthu . M’nthawi ya Samueli , Aisiraeli anagonjetsedwa ndi Afilisiti . 24 : 33 . Asayansi ochuka poyamba anali kukana kwa mutu wagalu kuti iyai . Kodi nafenso sitingatsegulile khomo anthu ocokela ku maiko ena amene ndi “ abale ndi alongo athu m’cikhulupililo ” ? — Mac . 14 : 27 ; Agal . Kodi anthu ambili amaciona bwanji cipembedzo ? ( a ) Ni mavuto ati amene anthu ambili a Yehova amakumana nawo ? Kodi akulu - akuku a boma la Aroma anaziona bwanji ziphunzitso zimene Paulo anali kulalikila ? Koma pa nthawiyi , Yehova sanamuuze kuti amenye thanthwe . Webusaiti yathu ya jw.org , imene pamapezeka zofalitsa m’zinenelo zambili , imathandizanso anthu kuphunzila Baibo . Mofanana ndi mboni zimene zimapeleka umboni m’khoti , anthu a Yehova anali ndi udindo wopeleka umboni wakuti Yehova ndi Mulungu yekha woona . ( a ) Kodi anthu ambili m’dzikoli ali na maganizo anji pa nkhani ya kugonana ? Coipa kwambili n’cakuti iwo anayamba kukopa Akhiristu anzawo kuti nawonso azicita zimenezo . Satana amafuna kusoceletsa otsatila a Yesu kuphatikizapo inuyo . Debora anawauza lonjezo la Mulungu lakuti adzagonjetsa Sisera ndi magaleta ake 900 . Ndi mmenenso moyo umakhalila nthawi zina . ( Ŵelengani 2 Akorinto 2 : 6 - 8 . ) M’bale Mumba : Cabwino , mwina tingaŵelenge lemba lina limene limveketsa bwino nkhaniyi . Ndipo ziyeneletso zina zipezeka pa Tito 1 : 5 - 9 , ndi pa Yakobo 3 : 17 , 18 . Mwacitsanzo , tonse tiyenela kuteteza zikhulupililo zathu , kulamulila mtima wathu , kukaniza ziyeso , kupewa mabwenzi oipa , ndi zosangulutsa zoipa . Ni mafunso ati amene mungadzifunse ngati mwamuna kapena mkazi wanu akukuikilani malile pa nkhani ya kulambila ? ( Luka 8 : 49 - 56 ) Ndiponso ziyenela kuti zinali zokondweletsa kwambili kwa khamu la anthu , limene linaona Lazaro akutuluka m’manda wamoyo , ndipo ali bwinobwino . — Yoh . Limbikilani pa kuthandiza ana anu kukulitsa makhalidwe ao acikristu . ( 2 Pet . Nanga tingapewe bwanji kutengela makhalidwe oipa a anthu a m’dzikoli kuti tipitilize kucita zinthu zokondweletsa Yehova , Mulungu wathu wa cikondi ? ( Sal . 40 : 8 ) Ana anu akayamba kudzimva motelo , adzadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizika . Anacita zimenezi kuti mu nthawi zimene zikubwela padzasonyezedwe cuma copambana ca kukoma mtima kwake kwakukulu kumene anatisonyeza mogwilizana ndi Khristu Yesu . ” — Aef . A Daka : Koma ngakhale kuti anthu sadziŵa dzina la Mulungu kapena kuligwilitsila nchito , io amam’dziŵabe kuti ndi Mulungu . Ngakhale kuti dilaiva winayo ndiye anali wolakwa , anayamba kunyoza Luigi na kufuna kumumenya . Musaiŵalenso kuti iye anapeleka Mwana wake kaamba ka anthu onse , kuphatikizapo mwana wanu . Ngakhale kuti Yehova anali ndi mtundu wosankhidwa padziko lapansi , iye sanaletse anthu amene sanali Aisiraeli kukhala pakati pa anthu ake . ( Miy . 27 : 11 ) Tikamaunjika ‘ cuma cathu kumwamba , ’ timakhala osangalala podziŵa kuti tacita zimene iye amafuna . ( Mat . Kuti acite zimenezi , anayamba kuŵelenga Baibulo ndi buku la Insight on the Scriptures . Cinyengo Kodi Cidzatha ? Ndimaona kuti ndinapanga cosankha cabwino kwambili paumoyo . ” Pakuti n’capatali kuti munthu wina afele munthu wolungama . Zoonadi , mwina wina angalimbe mtima kufela munthu wabwino . Onani kuti Marita sanakambe kuti : ‘ Nili na ciyembekezo cakuti mlongosi wanga adzauka . ’ Anadziŵa kuti Baibo ikhoza kukhala cida coopsa m’manja mwa munthu woopa Mulungu . Ganizilani mmene mumacitila panthawi zovuta . Kudzela mwa Debora , Yehova analamula kuti : “ Mukasonkhane paphili la tabori . ” N’nalandila Coonadi Olo Kuti Nilibe Manja ( B . Iye anali ataukitsidwa ndipo anapatsidwa ulemu . Ulosi wa m’Baibo umenewu komanso ena anakambilatu kuti Ufumu wa Mulungu udzaloŵa m’malo mwa maulamulilo onse a anthu na kubweletsa bata ndi mtendele padziko lapansi . Iwo anatilola kuti tikhale mbali ya gulu ili lomwe ndi logwilizana kwambili . M’Mabaibulo ambili , mulibe dzina lenileni la Mulungu . Zinali zacisoni kuona M’bale Knorr akuvutika na matenda a khansa mu 1976 . Lemba la 1 Akorinto 13 : 4 - 8 , lifotokoza mbali ziti za cikondi ? Iye anati : “ Munthu akafa , kodi angakhalenso ndi moyo ? ” — Yobu 14 : 14 . Conco , Paradaiso padziko lapansi ni cinthu cimene “ Mulungu amene sanganame , analonjeza kalekale . ” 3 : 19 ) Aliyense mumpingo amandithandiza ndipo amandikonda . N’navomela phunzilo la Baibo . Kodi nchito imene Mulungu anapatsa Adamu idzakwanilitsidwa motani ? Iye amadela nkhawa anthu amene akuvutika cifukwa ca matenda . N’zomveka kuti tingakhale ndi mafunso ambili ponena za moyo m’dziko latsopano . Ndipo “ Adamu anacha mkazi wake dzina lakuti Hava , cifukwa anali kudzakhala mai wa munthu aliyense wamoyo . ” ( Gen . Nafenso tingapambane ngati tilimbikila kugonjetsa zofooka zathu . “ Ndinayesako kuŵelenga Baibulo koma sindinalimvetse . Mphamvuyi imatithandiza kupanga zosankha mwanzelu ndi kuyembekezela mwacidwi zinthu zabwino . Tsopano nazindikila cifukwa cake Yehova amadana ndi zinthu zimene n’nali kukonda kwa nthawi yaitali . Tikamaganizila mfundo za m’Baibo posankha zocita , cikumbumtima cathu cimatitsogolela bwino , cifukwa cimakhala cogwilizana kwambili na maganizo a Mulungu . ( 1 Samueli 18 : 1 - 3 ) Yonatani anakhalabe wokhulupilika kwa Davide kwa moyo wake wonse . Caciŵili , lemba la Miyambo 18 : 1 limati : “ Wodzipatula amafunafuna zolakalaka zake zosonyeza kudzikonda . Cifukwa panthawiyo , Yesu anayamba kulamulila kumwamba osati padziko lapansi . Ndiyeno kumwamba kunayambika nkhondo . “ Kufatsa ndi kudziletsa . ” N’taŵelenga nkhanizo , n’nalimbikitsidwa kwambili . Kunena zoona tidzamusoŵa kwambili M’bale Pierce . A Daka : Ndithudi . Iye anakamba kuti pa cikhulupililo cathu , tifunika kupitiliza kuwonjezelapo kudziŵa zinthu , kupilila , ndi kukhala odzipeleka kwa Mulungu . — Ŵelengani 2 Petulo 1 : 5 - 8 . Kodi Muli pa Ubwenzi Wolimba ndi Yehova ? Fotokozani mmene ciphunzitso conama cinayambila kuloŵa m’Cikhiristu coona . Mofanana ndi ming’alu imene ingacititse kuti nyumba igwe , madandaulo ndi mkwiyo zikayamba kukula mumtima mwathu , zingacititse kuti kukhale kovuta kwambili kukhululukilana . Kodi anthu amene amakhulupilila Yesu adzapeza madalitso otani ? Zimakhala na phindu ngati ana amadziŵa zitundu zingapo . Mau a Mulungu amatitsimikizila kuti ngati timam’kumbukila ‘ m’njila zathu zonse , iye adzaongola njila zathu . ’ — Miy . M’malomwake , tiyeni tipitilize kukonda kwambili Yehova , Mau ake , ndi abale athu . 10 : 24 , 25 ) Zikondwelelo za pacaka ndi misonkhano ina zinalimbitsa Aisiraeli mwa kuuzimu . Musalole kuti anzanu akulepheletseni kukwanilitsa zolinga zanu . Yesu anali atapatsa otsatila ake nchito . Anati : “ Mudzakhala mboni zanga mu Yerusalemu , ku Yudeya konse ndi ku Samariya , mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ” 23 : 14 . Mulungu amaona zinthu zopanda cilungamo zimene zikucitika , ndipo adzazithetsa . — Mlaliki 5 : 8 . N’zosavuta kupeza mbali imene mufuna m’caputala cimodzi m’malo mofufuza mpukutu wonse monga wa Yesaya umene uli ndi macaputala 66 . Adziŵikitseni kwa ena kuti akhale omasuka . N’ciani cingatithandize kuti tipitilize kumvetsela mau a Yehova ? Ofalitsa amene anapita kukatumikila ku Turkey , tsiku lililonse amapeza anthu amene sanamveleko za Yehova . Elizabeth anam’yankha mafunso ake poseŵenzetsa Baibo . ( Genesis 12 : 10 - 13 ) N’cifukwa ciani Abulahamu anapempha zimenezi ? pangano la Cilamulo . 12 , 13 . ( a ) Kodi Satana anaonetsa bwanji kuti ndi wankhanza Yesu atabadwa ? Ngakhale kuti okwatilana angakhululukilane ndi kuthetsa mavuto m’banja lao , Baibulo limakamba kuti mwamuna kapena mkazi wosalakwayo ali ndi ufulu wosankha kaya kukhululukila kapena kuthetsa cikwati ndi mnzake amene wacita cigololo . ( Mat . Tiyeni tikambilane njila ziŵili za mmene Baibo imatithandizila kukhala na ciyembekezo codalilika ca m’tsogolo : 1 Imatithandiza kukhala na umoyo waphindu , ndipo 2 imatiphunzitsa mmene tingapangile ubwenzi wosatha na Mlengi wathu . Miyambo 24 : 16 imati : “ Wolungama akhoza kugwa ngakhale nthawi 7 ndipo ndithu adzadzukanso . ” N’cifukwa ciani sitifunika kumuyopa Satana na ziŵanda ? Maria anathaŵa . Ndiponso dziŵani kuti ana anu acinyamata salinso ana aang’ono . * Pa nthawiyo , Mtsogoleli wawo Khristu anali atatsala pang’ono kuphedwa , koma iwo sanali kumvetsetsa zimenezi . Ngakhale kuti anthu amene amakamba Cituvalu ndi ocepa poyelekezela ndi zinenelo zina , io afunikabe kulandila uthenga wabwino m’cinenelo cao . ” ( Aheberi 13 : ​ 20 , 21 ) M’nkhani ino , tikambilana zinthu zitatu mwa zinthu zabwino zimenezi : ( 1 ) zida zimene tapatsidwa , ( 2 ) njila zimene tagwilitsila nchito , ndiponso ( 3 ) maphunzilo amene talandila . Sankhani Baibo yodalilika ndi ya mau osavuta kumva . 19 : 4 , 5 , Buku Lopatulika ) Cimene Mulungu anapangila mkazi kucokela ku nthiti ya mwamuna n’kufuna kuti aŵiliwo aone umodzi wawo . Baibulo linakambilatu kuti : “ Uthenga wabwino uwu wa Ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” — Mateyu 24 : 14 . A Daka : Tiyenela kukhulupilila . Mmene amuna angatengele citsanzo ca Yesu . N’cimodzimodzi masiku ano . Tonse tifunika kudzipenda kuti tione ngati pali zinthu zina zimene zikutilepheletsa kutumikila Mulungu mokwanila . Kenako “ anaona malawi amoto ooneka ngati malilime , ndipo anagawanika ndi kukhala pa aliyense wa io limodzilimodzi . Ndiyeno onsewo anadzazidwa ndi mzimu woyela ndipo anayamba kulankhula zinenelo zosiyanasiyana , monga mmene mzimuwo unawacititsila kulankhula . ” ( Mac . ( b ) Nanga pemphelo limene mkulu angapeleke lingamukhudze bwanji wophunzila ? ( Mateyu 25 : ​ 31 , 32 ) N’cifukwa ciani abusa akale anali kulekanitsa nyama zimenezi ? Koma munthu amene wadzipeleka kwa Mulungu amanyadila kukhala wa Mboni za Yehova , ndipo amaonetsa zimenezi mwa kukhala ndi khalidwe loyela . Ana amenewo anayamba kufooka mwauzimu cifukwa cosamvetsetsa bwino tanthauzo la Mau a Mulungu . — Neh . 3 : 17 , 18 ) Inde , kwa caka conseci , tiyeni tizikumbukila mwacisangalalo zinthu zonse zabwino ndi kutsatila malangizo amene ali m’lemba lathu la caka ca 2015 , limene limati : “ Yamikani Yehova , cifukwa iye ndi wabwino . ” — Sal . Ndinawayankha kuti : “ Pa Yesaya 43 : 12 . ” N’ciani cingakuthandizeni kuonjezela ndi kulimbitsa cikhulupililo canu ? Kuti liyambe kugwila nchito , coyamba Yesu anafunikila kukhetsa magazi ake . Mwacionekele , Marita anali na zifukwa zomveka zomupangitsa kukhulupilila kuti mlongosi wake wokhulupilika , Lazaro , “ adzauka pa kuuka kwa akufa m’tsiku lomaliza . ” Yehova analamula angelo kuti azilangiza , kuthandiza , ndi kutsogolela Mose . 10 , 11 . ( a ) Kodi tingatsatile bwanji citsogozo ca Mulungu ? Mwini munda wa mpesayo anawafunsa kuti : ‘ Nakupatsani malipilo amene tinapangana , si conco ? 6 : 9 , 10 ) Zimenezi n’zinthu zabwino ngako zimene munthu angayembekezele . Pambuyo pake ndinagwilizana ndi mpingo umene unangokhazikitsidwa kumene ndipo unali kugwilitsila nchito cinenelo camakolo anga . N’ciani cinacitika Yesu atakumana ndi munthu wodwala khate ? Mwina mungaganizile za nkhondo , kuonongeka kwa zacilengedwe , ciwawa , kapena ziphuphu . Jack anakamba kuti nthawi zina amasungulumwa kwambili . Sisera sanali kum’dziŵa Yaeli . Yesu anayamikila mayiyo kaamba ka cikhulupililo cake , ndipo anacilitsa mwana wake wamkazi . — Mateyu 15 : 27 , 28 . Iye anaganiza zophunzila zambili kwa Yesu wa ku Nazareti . ( Yoh . Iwo sakwatila , kukwatiwa kapena kubala ana . Lemba la Miyambo 19 : 17 limati : “ Wokomela mtima munthu wonyozeka akukongoza Yehova , ndipo adzam’bwezela zimene anacitazo . ” Sara ni wodziŵika m’Baibo kaamba ka cikhulupililo cake colimba . Koma sikuti cikhulupililo cake cinali mwa mulungu wa mwezi amene anthu ambili anali kulambila ku Uri . Paulo anaticenjeza kuti : “ Ucimo usakhale mbuye kwa inu , cifukwa simuli pansi pa cilamulo koma pansi pa kukoma mtima kwakukulu . ” Amene amati kulibe Mulungu amakamba kuti tsogolo lathu lonse lili m’manja mwathu . — Sal . Osonkhanawo anasangalala kwambili , ndipo ambili anagwetsa misozi yacisangalalo atalandila Baibulo latsopano . ( Aheb . 12 : 6 ) Cilango cimene Mulungu amapeleka sicikhala ca nkhanza . Ndiyeno , ananitumiza ku sukulu ya olemala yochedwa Birkenwerder , imene inali monga sukulu ya boding’i . N’zoona kuti nthawi zina zimakhala zovuta , koma kutumikila kosoŵa kumabweletsa madalitso oculuka . 89 : 14 ) Kodi boma la Mesiya limeneli lidzaipitsidwa ndi kucotsedwapo ? ( 1 Mbiri 28 : 9 ) Kodi zimenezi zingatheke bwanji kwa ife anthu opanda ungwilo ? N’cifukwa ciani tingakhale ndi cidalilo cakuti Yehova adzacita zinthu mwa cilungamo ndi mokhulupilika ? Iwo sakaikila zimenezi ngakhale pang’ono . Mwa njila imeneyi , mzimu woyela umakhala ‘ cikole ca colowa cao cam’tsogolo , ’ kapena kuti citsimikizo cakuti adzakhala kumwamba osati pano padziko lapansi . — Ŵelengani 2 Akorinto 1 : 21 , 22 ; 5 : 5 . Damaris anati : “ Ku nchito kwathu kumabwela maloya kaŵili - kaŵili . “ AWILIWO ADZAKHALA THUPI LIMODZI . ” 31 : 12 . Njila imeneyi yopezela ndalama imapangitsa kuti akuluakulu ena a boma aziba ndalama . Mofananamo , ngati mwakukila mu mpingo wina , mukhoza kumakhala womangika . Kuti tikhale acimwemwe , tifunika kudziŵa Mulungu ndi kum’tumikila mokhulupilika . Ndiyeno , Gehazi anathamangila Namani mwakabisila , ndi kukamba zabodza kuti apemphe “ talente imodzi ya siliva ndi zovala ziŵili . ” ( Aheb . 12 : 2 ) Kuti tionetse kuyamikila cisomo cake , tiyenela kupitiliza kulimbitsa cikhulupililo cathu mwa kupemphela na kuphunzila Mau a Mulungu . — Aef . Kodi malemba amenewa atiphunzitsa ciani ponena za mmene Mulungu amaonela zinthu ? Makolo acikhristu amaona moyo wauzimu wa ana awo kukhala wofunika ngako kuposa zofuna zawo . — w17.05 , peji 9 - 11 . Otsatila a Wycliffe ochedwa kuti a Loladi anali ofunitsitsa kuthandiza anthu wamba kuti Mau a Mulungu awafike pamtima . Iwo anali kuyenda m’midzi yosiyana - siyana m’dziko lonse la England kukalalikila . Koma bwanji ngati m’bale wobatizika kapena mlongo wathaŵitsana ndi mwamuna kapena mkazi wa mwiniwake n’kukakwatilana , kenako n’kusudzula mnzake wa m’cikwati ? 34 : 10 - 12 . Kodi n’cinthu canzelu kupanga zosankha zokhudza banja lathu kapena nchito yathu popanda kufufuza coyamba mfundo za m’Baibo ? Nanga munthu angapilile bwanji cisoni ? Pelekani citsanzo . ( b ) Nanga ndi njila iti imene woyang’anila woyendela wina anapeza kukhala yothandiza ? Mau amenewa apezeka kaŵili mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika . ( Aef . 15 , 16 . ( a ) Kodi kusinkhasinkha za Yehova ndi Yesu kwakupindulitsani bwanji ? Ndipo wolemba mbili yakale waciyuda wochedwa Philo , anaonjezela cocitika cacinai . ( b ) Kodi tidzapeza mayankho pa mafunso ati ? 3 Kodi Mukumbukila ? Imeneyo ndi nchito ya Yehova . Kaamba ka ici , iye amagwila nchito mwakhama n’colinga cakuti anthu a Mulungu monga gulu akhale otetezeka olo kuti akukhala m’dziko loipa . Musalole kuti Satana akulefuleni kapena kukulepheletsani kukhala wokhulupilika kwa Mulungu mwa kukuwopsezani . ( Yoh . 14 : 12 ) Mwa ici , anawaphunzitsa mokwanila , cakuti analalikila uthenga wabwino m’dziko lonse lodziŵika panthawiyo . — Akol . 15 : 53 , 54 ) Imfa sidzakhalanso ndi mphamvu kwa aja amene adzaukitsidwa ku moyo wa kumwamba . Kodi tingam’cilikize bwanji Yehova pankhani ya ulamulilo ? Ndinali kudela nkhawa kuti makolo anga adzamva bwanji ndikapita kukatumikila kutali . Pokamba za “ mapeto a nthawi ino , ” Yesu Khiristu anacenjeza ophunzila ake kuti : “ Khalani maso , khalani chelu , pakuti simukudziŵa pamene nthawi yoikidwilatu idzafika . ” Komanso aliyense akamaona kuti onse m’banjamo amakonda kukamba za coonadi ndi kuti amakonda Yehova ndipo amafuna kum’kondweletsa , ubwenzi wao umalimba . ( Ŵelengani Yuda 4 . ) Pokhala Mwana wa Mulungu , iye alinso ndi mphamvu zothandiza anthu amene amafuulila Mulungu pofuna thandizo . — Ŵelengani Salimo 72 : 8 , 12 - 14 . Patapita zaka pafupifupi 300 Yesu atabadwa , Mfumu ya Roma yochedwa Diocletian inalamula kuti Mabaibulo onse aonongedwe . Koma pasanapite nthawi yaitali asilikali anadziŵa zimene zinali kucitika . Iye anakamba kuti poyamba zimene zinacitikazo zinamukhumudwitsa . Pamene anaima kuti apumuleko , mtumwiyo anapeleka malangizo akuti asapitilize ulendowo . Tinafunsako alongo angapo amene anatumikilapo ku maiko acilendo . ( Mateyu 6 : 13 ) Alona anati : “ Nthawi zonse belo locenjeza likalila , ndimapempha Yehova kuti andithandize kukhazika mtima pansi . ( Mateyu 24 : 45 - 47 ) M’caka cimeneco , anthu a Mulungu anamasulidwa ku ukapolo wophiphilitsila wa Babulo Wamkulu . Tsiku lina , ndinaganiza zopezekapo . Wotsutsa wina pa gululo sanapite patali na mtsutso wake atamuyankha mafunso ake poseŵenzetsa Malemba mwaluso . ( Aheb . 11 : 24 ) Mose sanaganize kuti angatumikile Mulungu m’nyumba yacifumu ndi kugwilitsila nchito cuma cake kuthandiza abale ake Aisiraeli . Kupatulapo mpatuko , pali zinthu zina zimene zingaononge mtendele wa mpingo . ( Onani pikica pamwambapa . ) ( b ) Tidzakambilana ciani m’nkhani ino ? Nsanja imeneyo inakamba kuti pamene mapeto a dzikoli ali pafupi kwambili , “ padzakhala zinthu zambili zosokoneza . ” Mofanana ndi wamasalimo , Paulo nayenso anapeza mphamvu mwa kuganizila mmene Yehova anali kum’thandizila nthawi zonse . Ngati mukukumana na ciyeso monga cimene Kim anakumana naco , mungacite bwino kuganizila mozama nkhani ya mnyamata wopanda nzelu wochulidwa pa Miyambo caputa 7 . ( b ) Nanga Yesu anaphunzitsa otsatila ake kupempha zinthu ziti ? Mabanja aŵili a Mboni na amene anali kutiphunzitsa Baibo anafe , cakuti 11 a ife tinakhala Mboni . Anthu onse odzipeleka kwa Yehova ali ndi mwai wochedwa mabwenzi ake ndiponso “ anchito anzake . ” Mofananamo , mphunzitsi masiku ano afunika kupatula nthawi yoceza ndi wophunzila kuti io akhale mabwenzi ndiponso kuti wophunzilayo akhale womasuka . M’malo mocita nkhondo , Agibeoni anacita pangano la mtendele ndi Aisiraeli . Koma Mulungu amafuna kuti tizitsatila Mwana wake mmene tingathele . Baibo inauzilidwa ndi Mulungu . Koma sikuti nchito yomasulila Mabaibo monga Septuagint , Wycliffe , King James Version , ndi Mabaibo ena ocita kumasulidwa , inauzilidwa mwacindunji ndi Mulungu . Mwacibadwa , timada nkhawa tikafuna kucita zinthu zina monga poyamba kulemba mayeso , pofunsidwa mafunso oloŵela nchito , ndi poyembekeza zotulukapo zake . Koma olo lelo litakhala tsiku langa lothela , nidziŵa kuti nidzaonananso naye mnzanga [ Don ] m’Paradaiso . Kodi Mose anali ndi umoyo wotani ali mnyamata ? Ndife otsimikiza mtima kuti ngati titsatila zimene Baibulo limakamba , tikhoza kusamalila zosoŵa za banja lathu Mau a mkuluyo ananithandiza maningi . ” — Mat . Malangizo amenewo sanawalande ufulu mwanjila ina iliyonse . — Ŵelengani Genesis 2 : 15 - 17 . Komabe , si ana onse amene amafunitsitsa kucita Kulambila kwa Pabanja , ndipo kunena zoona ena samasangalala . Ponena za nchito yathu yolalikila , n’ciani cimacititsa anthu ambili kukhulupilila kuti ndife Akristu oona ? Koma Yehova anatiumba ndi kutithandiza kusintha , ndiye cifukwa cake tili ndi makhalidwe abwino . Sitiyenela kulalikila cabe , koma tiyenela kuphunzitsa ndi kupanga ophunzila . — Mat . M’malo mwake , iye anali kuwalemekeza , kuwayamikila pa zabwino zimene anali kucita , ndi kuwaonetsa kuti amawakhulupilila . ( Luka 22 : 31 , 32 ; Yoh . Daniel analeledwa m’banja lokonda za cipembedzo ku Ireland . Ena apanga masinthidwe otani cifukwa ca kusintha kumene gulu lapanga ? * Ophunzila a m’kalasi ina ya Sukulu Yophunzitsa Baibo ya Akristu Ali Pabanja anayamikila kwambili maphunzilo amene analandila . Iwo anati : “ Maphunzilo apadela amene talandila akulitsa cikondi cathu pa Yehova ndipo ndife okonzeka kukathandizanso ena . ” Nyengo ya Cikumbutso : Ndi nthawi imene Cikumbutso cili pafupi kucitika , pamene cikucitika , ndiponso citangocitika kumene . * Koma cifuno cathu cinali cakuti tonse tikhale mu utumiki wanthawi zonse . Nkhondo itatha , atate anga anaikidwa m’ndende cifukwa boma linali kudana ndi maganizo ao pa zandale . Aliyense amene akanalephela kucita zimenezo anayenela kuponyedwa m’ng’anjo yoyaka moto . ( Mateyu 5 : 8 ) Kodi tili pakati pa anthu amenewo ? Athandizeni kupeza anzawo atsopano mwa kupanga makonzedwe akuti muzikhala na maceza olimbikitsa . Kukhala na cifundo cacikulu kudzatilimbikitsa kucitila ena zinthu mokoma mtima . Wolemba mbili yakale Heinrich Graetz , analemba kuti nduna za mfumuyi “ zikapeza mipukutu ya Cilamulo zinali kuing’amba ndi kuitentha . ” Analembanso kuti nduna zimenezi “ zinali kupha anthu onse amene anali kuŵelenga malemba kuti apeze citonthozo ndi cilimbikitso . ” Iye amakuphunzitsani mfundo za m’Baibo zimene mungagwilitsile nchito mosasamala kanthu ndi mmene zinthu zilili paumoyo wanu . Iye walonjeza kuti posacedwapa boma la Ufumu lidzayamba kulamulila dziko lapansi . Ndipo a zaka zopitilila 65 ciŵelengelo cawo cinawilikiza katatu . Conco , pamene Yosefe anapempha mtembo wa Yesu , Pilato anayamba ‘ kukayikila ngati [ Yesu ] anali atamwalila kale , conco anaitanitsa kapitawo wa asilikali ndi kumufunsa ngati iye anali atamwalila kale . ’ Yesu ndi Mfumu yoyenelela cifukwa ndi wacifundo . ( 2 Tim . 3 : 16 , 17 ) Kulalikila mogwila mtima sikumadalila pa ciŵelengelo ca malemba amene taŵelenga , koma mmene timawafotokozela malembawo . Cikondi — Khalidwe Lamtengo Wapatali , Aug . M’nthawi ya Oweluza , Aisiraeli mobweleza - bweleza anali kusankha mopanda nzelu . Koma mwina mungafunse kuti ‘ Kodi zimenezi zimathandiza bwanji ? ’ ( Yes . 6 : 8 ) M’bale Ralph Leffler anakamba kuti “ Tsiku limenelo linali ciyambi ceni - ceni ca nchito yolengeza Ufumu imene yafalikila padziko lonse lapansi . ” Ndi njila ina iti imene tingaonetsele Yehova kuti timam’konda ? Iye anali ataweluzidwa kuti apike ndende kwa zaka 25 . Paulo anali kufuna kuti Akhiristu a ku Efeso aziyesetsa ‘ kusunga umodzi mwa mzimu . ’ Ici ndiye cinali ciyambi ca kagulu ka akulu - akulu a chechi , ngakhale kuti Yesu anali atauza otsatila ake kuti : “ Nonsenu ndinu abale . ” Okwatilana angakhale ndi banja lolimba ndi lacimwemwe cifukwa ca thandizo la Yehova . 11 : 2 , 3 ) Inde , pansi pa Mutu wake , Yehova Mulungu , Khiristu Yesu wosaonekayo ndi waulemelelo anali kutsogolela mpingo . Iye anati : “ Ndinali kuopa kuti ndingadwale kansa ya m’mapapo . Ndinaopanso kuti ana anga angadwale . Kukamba zoona , pa mphatso zonse , palibe imene tingaiyelekezele na mtengo wa dipo umene sitingakwanitse kuufotokoza . 14 PARADAISO PADZIKO LAPANSI — NI YENI - YENI KAPENA NI MALOTO CABE ? Kuti mudziŵe zimene Baibulo limaphunzitsa ponena za akufa ndi ciyembekezo cimene ali naco , onani nkhani 6 ndi 7 m’buku lakuti Zimene Baibulo Imaphunzitsa . [ Mau okopa papeji 5 ] ( Maliko 7 : 9 ) Anthuwo sanali kucita khama kuti adziŵe tanthauzo la mau a Yesu . Odzozedwa apatsidwa nchito yolalikila “ ku mitundu yonse ” mapeto asanafike . Nanga apeza madalitso anji ? Iye analaka - laka kukhala monga namzeze amene anali na malo okhalitsa pa nyumba ya Yehova . Anakamba kuti : “ Inu Yehova wa makamu , ine ndimakondadi cihema canu cacikulu ! Koma kodi n’canzelu kusokoneza mgwilizano mumpingo cabe cifukwa ca cithandizo ca mankhwala ? ( Salimo 103 : 3 , 4 , 12 ) Yehova amatitsogolela ndi kutilangiza m’njila zosiyanasiyana . SATANA akucita nkhondo ndi odzozedwa ndiponso a “ nkhosa zina . ” Amatiuza kuti ndife mbali ya banja lake . Pambuyo poukitsidwa , Yesu anakhala yekhayo amene ali woyenelela kupulumutsa mtundu wa anthu . Conco , ndinabwelela kunyumba . ” — Aef . Wiki iliyonse , mkazi wanga anali kugwila nchito yochisa zovala za banja lina lake . Ngakhale kuti anthu ena sangaone nchito imene mumagwila , Yehova amaona Mwacitsanzo , timaŵelenga kuti cikondi “ n’coleza mtima ndiponso n’cokoma mtima . ” Kodi colinga cimodzi cimene Yehova anathandizila Danieli kukhala pa udindo wapamwamba cingakhale citi ? Titatumikila m’dela kwa zaka zinayi monga banja , anatiitana kukatumikila pa ofesi ya nthambi . Koma pochula makhalidwewa m’kalata yopita kwa Timoteyo , iye anaseŵenzetsa mau ena amene sapezeka kwina kulikonse m’Malemba Acigiriki Acikhristu . ‘ Tulilani Yehova nkhawa zanu zonse , pakuti amakudelani nkhawa . ’ — 1 PET . Mofananamo , mwina mukumbukila tsiku limene Mboni ya Yehova inakufikilani panyumba ndi kukulalikilani . Anthu a mumzinda umenewo anali okonda kulambila mafano na kucita zamizimu . Pofuna kuthetsa nkhaniyi mwamtendele , m’bale wina amene kumbuyoku anatumikilako monga mmishonale m’dziko limenelo anatumiwa kuti akaonane na Kazembe wa dzikolo ku London , m’dziko la England . Motelo , tiyeni tizidalila thandizo la mzimu woyela ndi citsogozo ca Atate wathu wakumwamba . Koma ndinalonjeza Yehova kuti ndidzapitiliza kusonkhana pambuyo pa miyezi itatu . Nthawi zina , anthu a Yehova anali kucita zopeleka zothandizila pa nchito zapadela . NKHANI YA PACIKUTO | KODI NDANI AMADZIŴADI ZAMTSOGOLO ? Akhiristu masiku ano , angalemekeze dzina la Yehova mwa kuteteza cikhulupililo cawo . Kapena munalandilapo magazini ino kucokela kwa mmodzi wa io . N’zoona kuti Yehova amafuna kuti atumiki ake ndi alendo azisangalala pamisonkhano . Musanasankhe njila iliyonse , muyenela kufunsa ku ofesi ya nthambi kuti mudziŵe njila zimene ndi zotheka m’dziko lanu . Amayi atamwalila , atate anapanga makonzedwe apadela na ahedi a pa sukulu pathu . Izi zitanthauza kuti muyenela kuika Yehova patsogolo pa ciliconse cimene mumacita mu umoyo wanu , kaya ni zokhudza maphunzilo , nchito , maudindo a m’banja , na zina zaconco . 6 : 22 . N’zoona kuti pambuyo pake Asa anacita zinthu mosaganiza bwino . MFUMU IPHUNZITSA ANTHU AKE KULALIKILA PADZIKO LONSE Kodi Yesu anayamba kugwila nchito yofunika iti pamene anali padziko lapansi ? Yeong Sug ndi mmodzi wa io . Ndipo ngati akulu ndi ololela ndi odzicepetsa , akapeza mfundo yoonetsa kuti afunika kusintha cosankha cawo , amasinthadi . 12 : 9 ) Satana anayambitsa nkhani yaikulu mwa kukamba kuti ana aumunthu a Mulungu analetsedwa kudya “ zipatso za mtengo uliwonse wa m’mundamu . ” Cina , Boazi anauza Rute kukhala pafupi ndi atsikana ake anchito kuti amuna amene anali kugwila nchito m’mundamo asamucite zacipongwe . 17 : 11 ; 1 Tim . 4 : 15 ) Sitifunika cabe kumvetsetsa mfundo zikulu - zikulu zimene zasintha , koma tifunikanso kumvetsetsa mfundo zonse , ngakhale zimene zingaoneke ngati zazing’ono . Ngakhale n’conco , anafunikila thandizo locokela ku maiko ena . Mwacitsanzo , monga mmene zimakhalila ndi anthu ambili amene anakumanapo na mavuto akulu - akulu , nayenso Ulf anaphunzila kukhala wacifundo ndi wokoma mtima . Cifukwa cakuti ambili saidziŵa bwino Baibo , ndipo ena saidziŵa n’komwe . Koma zimenezo zikanacititsa kuti cifunilo ca Mulungu cakuti ‘ dziko lidzaze ’ ndi ana omvela a Adamu ndi Hava cisakwanilitsike . Bwanji osakambilana zolinga zanu ndi ena mwa iwo ? Koma n’nacoka pa Beteli n’takwatila Angie . Kwa zaka pafupi - fupi zitatu , tinali kucita upainiya ku Staten Island . MASIKU ocepa Yesu ataphedwa , mtumwi Petulo anakumana ndi gulu la mphamvu la anthu otsutsa . ( a ) Tiyenela kupewa kuganiza ciani ponena za nkhani za m’Baibulo ? Musaleke kupita kumisonkhano kapena kuyanjana ndi mpingo . Kodi tingatsimikiziledi kuti malonjezo onse a Mulungu adzakwanilitsidwa ? N’namvela monga kuti nili m’banja lalikulu lokondana kwambili . M’nthawi ya atumwi , mkazi wina wacikhristu dzina lake Dorika anali kudziŵika ngako cifukwa ‘ cocita nchito zabwino , na kupeleka mphatso zacifundo . ’ Mwacitsanzo , mwina pa zocitika zina munadzionela nokha kuti Mulungu salola kuti tiyesedwe ndi zimene sitingapilile . Davide analemba kuti ‘ sinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa , kapena ana ake akupemphapempha cakudya . ’ Mogwilizana ndi ulosi , anthu masiku ano acita kunyanya pa nkhani yokhala osayamikila . ( 2 Tim . Tifunika kuyesetsa kucitila abale athu zinthu zabwino ‘ mwamseli , ’ kapena kuti mosadzionetsela kwa ena . Paulo anaona kuti ena mwa anthu amene anali kuwalalikila anali na makhalidwe monga amene iye anali nawo poyamba . Jowana anali mmodzi wa akazi amenewo . — Mat . Suona mavuto monga mwayi wothetsela cikwati . ” — Micah . Kuti mphatso ikhale yako , umangofunika kutambasula dzanja ndi kuilandila . 119 : 105 ) Pamene tivutika , tingatonthozedwe ndi malonjezo monga akuti : “ Inu Mulungu , simudzanyoza mtima wosweka ndi wophwanyika ” ndi akuti “ Kukoma mtima kwanu kosatha , inu Yehova , kunandicilikiza . ” Nkhani yake inali yokhudza “ mtembo wa Mose . ” Kodi zida zosiyanasiyana zatithandiza bwanji pa nchito yathu yolalikila ? Koma n’zacisoni kuti mumpingo wacikristu woyamba pang’onopang’ono munaloŵa mpatuko . ( Mac . Cocitika cimeneco cinali cabe ciyambi ca nkhondo ya Mfumu yokagonjetsa adani ake . ( Aheb . 6 : 10 ) Mbili ya kuwoloŵa manja kwake inalembewa m’Mau a Mulungu monga citsanzo cabwino cimene ise tonse tiyenela kutengela . Ndipo watitsimikizila kuti Mau akewo adzakhalapo mpaka kale - kale . 2 : 9 , 10 ) Nanga bwanji za Akhristu ambili okhulupilika amene ali na ciyembekezo codzakhala na moyo kwamuyaya pa dziko lapansi ? Nayenso Kelsey anati : “ Nikakhala na nchito yakuti nicite , n’nali kuzengeleza mpaka nthawi yocita nchitoyo itatsala pang’ono kutha . Cifukwa cakuti timayamikila “ mphatso za amuna ” zimenezi , ndipo timakonda Yehova ndi Kristu , Mutu wa mpingo . — Aef . Koma coyamba , tifunika kuyankha mafunso aya : Kodi Ophunzila Baibo anatenga kaimidwe kabwanji kulinga ku Babulo Wamkulu cikalibe kufika caka ca 1914 ? Ulosi wa m’Baibulo umatithandiza kukhulupilila kuti Yesu Kristu , Mfumu yathu ya kumwamba , posacedwapa ‘ adzaononga nchito za Mdyelekezi . ’ Ngati timakhala tokha , tingaphunzile nkhani za conco pa phunzilo laumwini . Ciwawa cinali ponse - ponse . N’cifukwa ciani tifunika kuthandiza ena kupita patsogolo ? Kodi lamulo la Yesu la pa Mateyu 28 : 19 , 20 lingawathandize bwanji makolo pamene akuphunzitsa ana awo ? 3 : 1 ) Conco , tingacite bwino kudzifunsa kuti , ‘ Kodi nimayang’ana kwa ndani nikafuna thandizo na citsogozo ? ’ Kuwonjezela apo , anacitapo kanthu pa zimene Alexandra anamuuza , ndipo anayamba kuphunzila Baibo . Mukaŵelenga lemba limeneli , kodi nanunso mumayamikila Yehova ngati mmene wamasalimo anacitila ? ( M’masiku amenewo , pa misonkhano ya cigawo anthu anali kupatsidwa cakudya . ) Kuwonjezela apo , amatisamalila mokhulupilika , monga mmene tate wacikondi amasamalila ana ake . Iwo angakuuzeni zosoŵa zapadela zimene ena sangadziŵe . DZIKO : GERMAN DEMOCRATIC REPUBLIC ( a ) N’ciani cingatithandize kukhala ocilimika kuti tipeze madalitso a Mulungu ? Aisiraeli anamwa madzi , ndipo vuto la kusoŵa madzi linatha . — Eks . Komabe , tili ndi mdani amene mwamacenjela angaononge mzimu wathu wodzimana . 5 , 6 . ( a ) N’ciani cimene Satana anacita kuti alepheletse cifunilo ca Mulungu ? Kodi pamakhala zotulukapo zotani ngati tipitiliza kulalikila ngakhale kuti ena akutizunza ? M’kupita kwa nthawi , adzayamba kukhulupilila zimene akuphunzila , ndipo adzakhala okonzeka kuteteza cikhulupililo cawo pamaso pa ena , kuphatikizapo anzawo a ku sukulu . ( 1 Pet . 132 : 7 ) Kacisi ameneyo anali kugwilitsidwa nchito monga malo olambililapo Mulungu woona . Nkhani ziŵilizi , zimene ndi zozikidwa m’buku la Levitiko , zidzafotokoza cifukwa cake Yehova amafuna kuti anthu ake akhale oyela , ndi mmene tingaonetsele khalidwe limeneli . 1 : 19 - 21 . Tiyeni tikambilane zimene zinacitika m’nthawi ya Debora ndi Baraki . Kukambilana zimenezi kudzatithandiza kuyankha mafunso amenewa . 22 : 37 . Mungasinkhesinkhenso pa malemba ndi zofalitsa zimene mufuna kukagaŵila . Iwo anali kusiya Yehova ndi kuyamba kutumikila milungu yonama . Mwacitsanzo , m’mau ake a patsogolo pa lemba la 2 Timoteyo 2 : 19 , Paulo anauza Timoteyo kuti “ asamakangane pa mau ” ndi kuti “ azipewa nkhani zopeka . ” Conco , kaya vuto n’lalikulu kapena laling’ono , tifunika kumvela malangizo a wamasalimo akuti : “ Lola kuti Yehova akutsogolele panjila yako , umudalile ndipo iye adzacitapo kanthu . ” — Sal . Kodi Mkhristu angacite ciani kuti apewe ciwelewele ? Kufatsa — Kumaonetsa Nzelu , Dec . Pofuna kugogomeza mfundo yake , Petulo anagwila mau a Davide a pa Salimo 110 : 1 . Koma iye anapempha Yehova kuti amuthandize kuthetsa maganizo olakwika amene anayamba kukhala nao mumtima mwake . ( Salimo 72 : 12 - 14 ) Baibulo limalonjezanso kuti : “ Palibe munthu wokhala m’dzikolo amene adzanene kuti : ‘ Ndikudwala . ’ ” Pa cisumbuco panali ofalitsa 20 cabe , ndipo cinali pa mtunda wa makilomita 9,000 kucokela kumene tinali kukhala . Zinthu sizinacitike monga mmene Mulungu anali kufunila . Pamene Adamu anauka , anakondwela kwambili ndipo anati , “ Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga ndi mnofu wa mnofu wanga . Lemba la Miyambo 19 : 18 limaonetsa kuti imeneyi ni nkhani ya moyo kapena imfa . Banja linanso la ku Germany linalembela kalata ku Ofesi ya Nthambi yoyamikila mmene abale a ku Ireland anawalandilila bwino ndi kuwasamalila pamsonkhano wacigawo kumeneko . Iwo anati : “ Tikuyamikila kwambili Yehova ndi Yesu Kristu , Mfumu imene iye anaika . 13 : 4 , 5 ) Kusungila munthu cakukhosi , kungawononge ubwenzi wathu ndi m’bale kapena mlongo wathu . Koma coopsa kwambili , kungawononge ubwenzi wathu na Yehova . ( Mat . Lolani kuti zimene mwaŵelenga zikukhudzeni mtima , ndipo yamikilani Yehova pa zinthu zabwino zimene wakuphunzitsani Yesu analangiza ophunzila ake mobweleza - bweleza kuti : “ Khalani maso . ” Tingakhale na mafunso ambili pankhaniyi . Tsopano mantha a Yehova akugwileni . Munthu wina amene anali kugwilizana ndi banja lathu anauza Amalume a Nick kuti akanipeleke ku sukulu ya ana ogontha . Conco amalume anakanilembetsa ku sukulu ya ogontha mumzinda wa Saskatoon , ku Saskatchewan . Tikambilananso zimene tingacite kuti maganizo ndi cikumbumtima cathu zizitithandiza kukhala okhulupilika ku Ufumu wa Mulungu . Panthawiyo , n’nali wocepa thupi kwambili ndipo n’nali kulemela makilogilamu 57 cabe . 92 : 1 , 4 ) Monga wacicepele , ganizilani zinthu zimene Yehova anakucitilani . Nanga tsopano akulu adzamuuza ciani ? M’malomwake , ndinayamba bizinesi yanga . Pambuyo pochula Malamulo 10 , ndi ena amene Yehova anapeleka , Mose anawakumbutsa mfundo yofunika kwambili imene ili pa Deuteronomo 6 : 4 , 5 . Sara analidi mlongosi wake wa Abulahamu , koma wa mimba ina . Tinasangalala kwambili pamene tinali kutumikila abale ndi alongo athu m’mipingo yosiyanasiyana . Yehova safuna kuti tizibwezela coipa , ndi kusunga cakukhosi . 65 : 2 ) Koma kodi timakonda kulankhula naye m’phemphelo kawili - kawili ? Onani mmene tapindulila ndi zikumbutso zimenezi m’zaka za posacedwapa . Monga mmene zinalili m’nthawi ya Yesu , masiku anonso mzimu wa tsankho ni wozika mizu kwambili . N’ndani amene Baibo imakamba kuti ni anthu a Yehova apadela ? Abale acinyamata a pa Beteli ndiwo adzakhala anzanga . ’ ” N’cifukwa ciani kuuka kwa Yesu kumatithandiza kuti tizilalikila molimba mtima ? Koma tifunika kusungabe ubwenzi wathu wamtengo wapatali na Atate wathu wakumwamba . 6 : 33 . Kupilila matenda aakulu Amene akuchulidwa kuti “ abale anga , ” ndi amuna ndi akazi odzozedwa amene adzalamulila ndi Kristu kumwamba . 24 : 42 . Umboni wakuti ali ndi mzimu woyela . 10 : 37 ) Tikumbukilenso kuti Satana angaloŵele ku cikondi ca pacibululu kuti awononge cikhulupililo cathu . Ciphunzitso ca utatu calepheletsa anthu oona mtima kutengela citsanzo ca Yesu Kristu , ndi kuti ayandikile Mulungu , monga mmene Baibulo limatilimbikitsila . — 1 Akorinto 11 : 1 ; Yakobo 4 : 8 . Zimacita miyambo ya zikondwelelo yogwilitsila nchito makandulo , kuimba nyimbo , kupemphela , ndi kucita zinthu zina . ‘ Anathamangitsabe adani ’ ao . — Oweruza 8 : 4 . M’Baibo mulinso malangizo ena othandiza . “ Inoki anasamutsidwa kuti asafe mozunzika . ” Ndinawauza kuti tidzakambilana malembawo ndi wansembe wa ku chalichi cathu . Kodi ndimakhululukila mwamsanga zolakwa za abale anga monga mmene ndimafunila kuti io andikhululukile ? Iwo anazindikila kuti Yehova amadana ndi anthu acinyengo , ndipo anali kuwaona akamakoka fodya . Komabe , liu lakuti asher lingamasulidwenso monga liu lofotokoza zotulukapo za cocitika cinacake . Mwacitsanzo , lingamasulidwe kuti “ moti , ” “ kotelo kuti , ” kapena “ ndiyeno . ” Ine na mmishonale mnzanga Raymond Leach tinayenda masiku 47 pa boti kupita ku Philippines Iwo anayesetsa kucita zimene akanatha kuti asakhumudwitse Mbuye wawo . Ngati munalabadila malangizowo na kusintha , muyenela kukondwela . Koma mau a Yesu a pa Mateyu 24 : 34 amatitsimikizila kuti odzozedwa a ‘ m’badwo uwu sadzatha onse kucoka ’ cisautso cacikulu cisanayambe . Sitiyenela kukamba kapena kucita zinthu zimene zingayambitse magaŵano ndi kulimbikitsa mzimu watsankho pakati pathu . — Aroma 14 : 19 ; 2 Akor . Baibo si buku longophatikiza pamodzi mabuku osagwilizana aciyuda ndi acikhiristu . Ngakhale kuti makolo ake anafa ndi matenda a kansa ya m’mapapo , iye anapitilizabe kukoka fodya , uku akulela ana ake aŵili . Aisiraeli ataona Mose , anacita mantha , cakuti Mose anaphimba nkhope yake na nsalu . ( Eks . N’ciani cimacititsa atumiki ena acangu a Yehova , monga mlongo amene tachula , kulefuka ? Kumbukilani kuti Paulo anadzimvela cisoni cifukwa colephela kumvela Yehova pa zinthu zina . Komabe , pambuyo pake iye anati : “ Mulungu [ adzandipulumutsa ] kudzela mwa Yesu Khristu Ambuye wathu . ” Iwo angakambe kuti : “ Zinthu zauzimu nimazikonda , koma sinifuna kuloŵa cipembedzo ciliconse . ” Kodi anthu amakumana ndi mavuto otani ? Ulosi umenewu udzakwanilitsikanso mtsogolo . Anthu okonda umoyo wofewa amenewa analangizidwa kuti ‘ aganizile ’ za mwayi wotumikila Yehova umene anataya . Mwacitsanzo , Msonkhano wa ku Nicaea utatha , Constantine , amene analipo pa msonkhanowo , anapitikitsa wansembe wina dzina lake Arius kuti acoke m’dziko lake cifukwa cokana kuvomeleza kuti Yesu ni Mulungu . Aka kanali koyamba kumvela kuti Mulungu ali na dzina . 28 Yehova Atamandike Cifukwa ca Kudzipeleka Kwanu ! Tingatsimikize bwanji kuti Mulungu sindiye amacititsa zinthu zoipa ? Angelo oipa anavala matupi a anthu na kudzitengela akazi , ndipo anabala viphona vankhanza . ( Gen . Wokwela pa hosi imeneyi akuimila nkhondo . Mwa kucoka mumpingo , zili monga anapita “ kudziko lina lakutali , ” limene ndi dziko la Satana lotalikilana ndi Yehova . ( Aef . 3 : 1 ) Kucita zimenezo ndi cinthu canzelu . Pambuyo pake , n’namva ululu ngati umene Baibulo imauyelekezela na ‘ lupanga lalitali lolasa moyo wako . ’ — Luka 2 : 35 Kunena zoona , Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse inasintha zinthu kwambili padzikoli . 24 : ​ 45 - 47 . Mu Salimo 118 , imene ena amaganiza kuti inalembedwa na Davide , muli pempho lakuti : “ Haa ! Mwacitsanzo , anthu oyambitsa mgwilizanowu ananena kuti analemba cipepala cao ca mgwilizano mosamalitsa kuti asakhumudwitse zipembedzo zina zimene zili mumgwilizano umenewu . Kodi cimeneci n’cilungamo ? ” Mwacitsanzo , pambuyo polalikila kwa nthawi yaitali ndi ophunzila ake , iye anawauza kuti : “ Inuyo bwelani kuno , tipite kwatokha kopanda anthu kuti mupumule pang’ono . ” — Maliko 6 : 31 , 32 . ( Mlaliki 9 : 5 ) Pophunzitsa , Yesu anayelekezela imfa ndi tulo tofa nato . Ngakhale Yesu sanatiuze kuti kapolo wake wokhulupilika adzayamba kutipatsa cakudya cauzimu cangwilo . Iye anasankhidwa ndi Yehova kuti aziyang’anila nkhosa zake . — Ŵelengani Yohane 10 : 3 - 5 . “ Tsopano , natumikila monga mpainiya m’tauni yathu kwa zaka 4 , ndipo nazindikila kuti n’nacita bwino kutsatila malangizo amene ananipatsa . Kodi izi zitanthauza kuti angelo sathandiza anthu ? Cinanso , popeza kuimba ni mbali yofunika pa kulambila kwathu , Bungwe Lolamulila linaona kuti buku la nyimbo lifunika kukhala lokongola , lacikuto colingana ndi ca Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso . Iye anati : “ Kwa zaka zambili zimene natumikila m’madela osiyana - siyana , n’nakhala na alongo a zikhalidwe ndi zibadwa zosiyana ndi ine . KOMA anthu ocilikiza mgwilizano wa zipembedzo amaona nkhaniyi mosiyanako . 11 : 28 ) Mose anadziŵa kuti Yehova ndi wokhulupilika , ndipo anakhulupilila lonjezo la Yehova lakuti adzapha ana aamuna oyamba kubadwa aciiguputo . Koma kodi Baibulo lingakuthandizeni inuyo kuyandikila Yehova ? Zili conco cifukwa cakuti Satana , mdani wa Mulungu amene amatsutsa ulamulilo wake , anatonza Yehova mwa kukamba kuti anthu onse amatumikila Mulungu cifukwa ca dyela cabe . Pambuyo pake ndinapatsidwa mwai wotumikila pa likulu la Mboni za Yehova ku Brooklyn , New York . Kuthandiza anthu ambili kudziŵa coonadi camtengo wapatali komanso copatsa moyo , kwaticititsa kukhala ndi cimwemwe cosaneneka . Kodi ana anu mukuwasiila citsanzo cotani kuti atsatile ? M’nkhaniyi tikambilana mfundo za m’Malemba zimene zidzatilimbikitsa kulemekeza malo amenewa ndi kupelekela ndalama zocilikizila nchito yomanga nyumbazi . Nthawi zina tikakhumudwitsana cifukwa ca kupanda ungwilo , M’bale Woodworth anali kukamba kuti , “ Zimene Ambuye acita n’zocititsa cidwi ngakhale kuti akuseŵenzetsa anthu opanda ungwilo . ” N’zoona kuti kungocokela pamene tinalengedwa , tinakhala anthu a Yehova , mofanana ndi anthu ena onse . N’zoona kuti Baibulo silikamba kuti tiyenela kukhala mpainiya kuti titumikile bwino Yehova . NYIMBO : 40 , 98 ( b ) Ni malingalilo abwanji amene makolo ena apelekapo ? Kodi udani umenewu unali kudzakhala waukulu motani ? Zimenezi zimandikhazika mtima pansi . ” Ifenso timayembekezela nthawi yosangalatsa imeneyo , ndipo ili pafupi kwambili . — Aroma 6 : 23 . Koma mwadzidzidzi umoyo wake unasinthilatu pamene masoka anatsatizana . Tikupemphani kuti muŵelenge nkhani yotsatila kuti mumve zina mwa mfundo zimenezi . Masiku ano , cizoloŵezi cimeneci m’madela ambili mulibe . Mwacitsanzo , kodi muona kuti n’copepuka munthu masiku ano kukhala mwamuna kapena mutu wa banja wabwino ? N’cifukwa ciani tifunika kumaganizila za kufunika kocilikiza ulamulilo wa Yehova ? Kukambilana pasadakhale ndi momasuka n’kofunika M’baleyo anamvetsela uphungu ndipo m’kupita kwa nthawi anagonjetsa cizoloŵezi coipa cimeneco . Mufunsanso kuti , “ Koma kodi cakhala cikutetezedwa ? ” Kodi kuona mtima kwawo kunawapindulitsa m’njila lililonse ? Cifukwa cotangwanika na zocitika pa umoyo , cingakhale cosavuta kuiŵala zinthu zofunika . ( Onani palagilafu 14 - 18 ) Funso lina n’lakuti , tingacite ciani kuti tizitha kudzilanga tekha ? PAMENE SAULI , mfumu ya Aisiraeli , anayamba ulamulilo wake , anali munthu wodzicepetsa ndi wopatsiwa ulemu . ( 1 Sam . Tsiku lina , n’napezekapo pamene azimayiwo anali kuphunzitsa anzangawo . ( Miy . 18 : 13 ) Ngati amakonda nkhani za sayansi , angafune kukambapo ukachula mmene Baibulo imakambila zoona za sayansi . Muziuza mkazi wanu maganizo anu ndi mmene mukumvelela . Sinkhasinkha zinthu zimenezi mozama . Dzipeleke pa zinthu zimenezi kuti anthu onse aone kuti ukupita patsogolo . ” — 1 Tim . Yesu anali kukhulupilila zimenezi , ndipo zimene anali kuphunzitsa zinathandiza anthu kukhala na cikhulupililo . Anadya cipatso coletsedwa cimene mkazi wake , Hava , anam’patsa . Ni mfundo zina ziti zimene zingatithandize kukulitsa luso lathu loimba ? ( Aroma 15 : 2 , 3 ) Yesu anaika zofuna za ena patsogolo , ndipo anali kukonda ngako kuthandiza anthu pocita cifunilo ca Mulungu . Nanga angacite bwanji phunzilo laumwini ? Zimene anacitazi zinapangitsa kuti zinthu zisinthe kwambili . Zinathandiza anthu ambili kukhalanso ndi cidwi na Mau a Mulungu . Uthenga Wabwino Wocokela kwa Mulungu Iwo anafunika kuŵelenga Cilamulo tsiku na tsiku , kucikopela , ndi ‘ kusunga mau onse a cilamuloco , kutinso azitsatila malangizo ake . ’ — Ŵelengani Deuteronomo 17 : 18 - 20 . Kuulula macimo na kuwaleka . Ataona pacikuto anandifunsa kuti , “ Kodi nawenso ufuna kukhala wa Mboni ? ” ( b ) nanga anamwali ndani ? Nanga n’ndani amene sanakhudzidwepo na matenda ndi imfa ? Khiristu wapatsa abale ake odzozedwa amene ali padziko lapansi “ utumiki wokhazikitsanso mtendele . ” Mfundo pamenepa ndi yakuti , tiziyesetsa kugwilitsila nchito njila zatsopano zolalikilila uthenga wabwino . N’ciani cinathandiza Paulo kupitiliza kukonda Mulungu ? Ena amakonda kupenyelela mafilimu aciwelewele , maseŵelo oipa , kapena mapulogalamu oipa a pa TV . Koma n’zomvetsa cisoni kuti m’kupita kwa nthawi , atate analeka kupezeka pa misonkhano yacikhristu cifukwa coika maganizo awo pa zophophonya za Akhristu anzawo . Kodi mungawathandize bwanji ana anu kukhala na nzelu zaconco ? Sitifuna kukhumudwitsa Yehova mwa kucita zinthu zimene iye amadana nazo . Ndinacoka panyumba ndili ndi zaka 18 . Apainiya aŵili ku Amsterdam akulalikila uthenga wa Ufumu kwa munthu wopita m’njila Mpake kuti Baibulo limafotokoza kuti ucimo ndi imfa zimene tinatengela zili ngati “ cophimba cimene cikuphimba anthu onse , ndi nsalu imene yakuta mitundu yonse . ” Koma Yosefe anali wophunzila wa Yesu ngakhale kuti anali kuopa kudzidziŵikitsa kuti anali wophunzila wake . Mboni zopanda mantha monga zimenezi zinapitiliza kulalikila uthenga wabwino mosamala m’cigawo ca kwathu , ku mpoto kwa Kyrgyzstan . Popeza panthawiyo tinali cabe ndi mwana mmodzi panyumba , dzina lake Debbie , inenso ndinayamba upainiya . ( Sal . 143 : 5 - 7 , 10 ) Pa nthawi ngati zimenezo , mungafunike kuyembekezela Atate wanu wakumwamba kuti akuonetseni cimene cili cifunilo cake kwa inu . Umoyo . Cikhulupililo cathu mwa Yehova cimakula tikaona mmene amatithandizila ndi mmene amayankhila mapemphelo athu . Ndinapempha Yehova ngati ndingapitilize kuphunzila naye kapena ai . Ndiyeno tsiku lina , mngelo wa Yehova anauza mkazi wa Manowa kuti adzakhala ndi mwana wamwamuna . Zekariya anali kudziŵa kuti Ayuda amene anacoka ku Babulo kupita ku Yerusalemu anali na cikhulupililo colimba . Baibulo lili ngati nyale yotiunikila njila imene tiyenela kuyendamo kuti zinthu zitiyendele bwino . Masiku ano , Yehova ndi Yesu amasangalala kwambili akaona paladaiso wathu wauzimu . Marilyn anati : “ Pamene ndinamva mfundo yakuti kulambila kwa pabanja kokhazikika n’kofunika kuti tikapulumuke tsiku lalikulu la Yehova , ndinaona kuti ndinafunikila kubwelela kunyumba . Nalonso lemba la Aroma 8 : 6 limafotokoza ubwino wokhala munthu wauzimu . Imodzi mwa njila zimene timalandilila malangizowo ni mwa kuŵelenga na kusinkha - sinkha nkhani za anthu ochulidwa m’Baibo . Baibulo limati , “ Asa anacita zabwino pamaso pa Yehova ” ndi kuti “ anatumikila Yehova ndi mtima wathunthu . ” Koma m’ma Baibo a Cizungu ambili masiku ano , dzinali mulibe . 3 Muziimba Mosangalala ! Iye anafotokozela atsogoleli acipembedzo a m’nthawi yake kuti : “ Ndinatsika kucokela kumwamba kudzacita cifunilo ca iye amene anandituma , osati cifunilo canga . ” N’cifukwa ciani nthawi imene tikukhala ni yapadela ? 32 Dzina la m’Baibo pa Mtsuko Wakale Anacita cigololo na Bati - seba . Koma m’kupita kwa nthawi , kuphunzitsa ena ndiye kumasungitsa nthawi . — Aef . Ahabu sanamvelenso lamulo la Yehova lakuti aphe Beni - hadadi , Mfumu yoipa ya Siriya . Monga Mulungu wadongosolo , Yehova amapatsa aliyense wa ife malo ake , kapena mbali yake , m’banja la Mulungu . Timaonetsa kuti timatsanzila kuolowa manja kwa Yesu mwa kupatsa ena zinthu zakuthupi ndi za kuuzimu ngati tingakwanitse . ( Luka 12 : 32 ) Kodi anthu a “ kagulu ka nkhosa ” ndi angati ? Coyamba , n’zolimbikitsa kudziŵa kuti Yehova amadziŵa bwino anthu okhulupilika kwa iye . Satana anagwetsela Yobu mayeselo aakulu . ( Gen . 18 : 25 ) Pofunsa funso limeneli , Abulahamu anaonetsa kuti anali kukhulupilila kuti Yehova adzaŵeluza molungama mizinda ya Sodomu ndi Gomora . Anthu oloŵa sukulu imeneyi angakhale apabanja , abale osakwatila , kapena alongo osakwatiwa . Panthawi ya Ulamulilo wa Zaka 1,000 , Yesu pamodzi na mafumu komanso ansembe anzake okwana 144,000 adzathandiza anthu okhulupilika kukhala angwilo . Aksamai anakhala mlaliki wokangalika wa uthenga wabwino . Onani zitsanzo zotsatilazi : Popeza n’nali wacicepele , sin’nali kuganizila kwambili za colinga ca moyo kapena za tsogolo . Ponena za ulamulilo wake , Baibo imati : “ Anacita zoipa . ” Panali patapita mlungu umodzi kucokela pamene bwenzi lao linawapatsa buku lonena za dziko la Nepal , ndipo io anali kuona kuti malowo ndi abwino kwambili kukacezako . Motelo mzimu wa Mulungu ndi mzimu wanu zimacitila umboni kuti muli ndi ciyembekezo cakumwamba . Vesi lina la nambala 6 pamene pakupezekanso dzina la Mulungu ndi pa Oweluza 19 : 18 , ndipo linaonjezeledwa pambuyo popenda mosamalitsa mipukutu ina yakale ya Baibulo . N’nabadwila m’tauni yokhala na anthu ambili yochedwa Paddington , mumzinda wa London , ku England . Tizikumbukila kuti mankhwala angathe kubweletsa mavuto aakulu ngakhale kuti anthu ambili amawagwilitsila nchito . — Ŵelengani Miyambo 27 : 12 . 25 : 34 - 40 . Ganizilani izi : Babulo Wamkulu ni ufumu wa dziko lonse wa cipembedzo conama . 3 : 18 . Yehova amafuna kuti cikwati cikhale cokhalitsa ndipo amafunanso kuti okwatilana azikondana . N’kosavuta kwa io kukondana akangoloŵa m’cikwati . Anati : “ Yehova wa makamu ndi amene muyenela kumuona kuti ndi woyela . ” ( Yes . Muyang’anilenso nsomba , . . . , zolengedwa zouluka . . . , komanso colengedwa ciliconse cokwawa padziko lapansi . ” ( Gen . Mungacite ciani ngati covala canu cada ndipo cayamba kununkha ? Mungacivule mwamsanga , si conco ? ( Yobu 34 : 10 ) N’zoona kuti makolo akhoza kuphunzitsa ana ao zinthu zabwino kapena zoipa . 1 , 2 . ( a ) Fotokozani cocitika cimene cionetsa phindu lofunsa mafunso oyenelela . Yehova anacha Sara kuti “ Mfumukazi , ” koma Sara sanayembekezele kucitilidwa zinthu monga mfumukazi Kodi Mulungu Angandithandize Ndikapemphela ? MIPINGO Conco , ngati sitilalikila kuti tipeze ndalama , kodi timalalikila cifukwa ca ciani ? N’takana , ananichaya makofi ndi kunimenya na ndodo . “ Malemba oyela ” amene Timoteyo anaphunzitsidwa ndi amai ake ndiponso agogo ake ‘ kuyambila pamene anali wakhanda , ’ anaphatikizapo malangizo othandiza kwa acinyamata . Zimene anayankha zinaonetsa mmene anali kumvelela pa nkhani imene inali kudzasintha umoyo wake . ( Zek . 4 : 10 ) M’kupita kwa nthawi , tikhoza kukhala ndi zosatilapo zabwino kwambili kuposa mmene tinali kuganizila poyamba . — Sal . ( 1 Akorinto 6 : 18 ) Pamenepo anazazuka kuti , “ Wati ciani ? ” N’cifukwa ciani tingakambe kuti gulu la Mulungu n’lapadela ? Kuceleza sikulila kukhala na zinthu zambili . Nimayelekezela kuti nikumuona tili limodzi m’munda wathu , ndipo nikumuonetsa cikondi ngati cimene n’namuonetsa atangobadwa . ” ( 1 Akor . 13 : 2 ) Koma kodi cikondi n’ciani ? Ndipo tingacitenji kuti tikhale naco ? N’ciani cinapangitsa mundawo kukhala wokongola kwambili ? Iye sanaikidwe pambuyo pobwelela kumwamba ataukitsidwa . Mwacitsanzo , Paulo anacenjeza abale ake kuvala “ codzitetezela pacifuwa cacikhulupililo ndi cikondi . ” ( 1 Ates . Zoona , iwo anafunikadi kumasuka . Ngati mwayankha kuti inde pa imodzi mwa mafunso aya kapena kuposapo , lomba ni nthawi yakuti mulimbitse cikwati canu . M’zinenelo zimenezo , mau akuti “ soul ” nthawi zambili amatanthauza mzukwa ( cipuku ) kapena cinthu cina cake cimene anthu amati cimacoka m’thupi mwa munthu akamwalila . Arthur Willis akukonzekela ulendo wokalalikila ku dela lakutali m’dziko la Australia . — Ku Perth , Western Australia , 1936 Anapitiliza kukhala mwamantha kwa zaka 20 kufikila pamene Yehova anaona kuti anthu ake ouma khosi anali kufuna kusintha . Kuti tilimbane na mavuto amenewa , pamafunika nthawi yoculuka , mphamvu , na ndalama zambili . Iye amamvetsela mapemphelo a anthu mamiliyoni ambili panthawi imodzi , mosasamala kanthu kuti akukamba cinenelo cotani . Kodi kudzicepetsa kumatanthauza ciani ? Iye anali kuidziŵa bwino imfa cifukwa anali kuona nyama zikufa . Kumeneko umoyo wake unasokonezeka kwambili cakuti anayamba kumwa amkola bongo , kumwa moŵa mwaucidakwa , na kucita zaciwelewele . Timadziŵa bwanji kuti Yesu sanatanthauze kuti tizibweleza mau a m’pemphelo lacitsanzo popemphela ? N’naphunzilanso kuseŵenzetsa zida pomenyana . ( b ) Nanga Paulo anaitsiliza bwanji nkhaniyo ? Komabe , mfundo imeneyi iutsa mafunso ena . Nanga imwe muli na zifukwa zanji ‘ zotamandila ’ Yehova pa umoyo wanu ? — Sal . ( a ) N’cifukwa ciani sitiyenela kuganiza kuti odzozedwa ambili a Kristu adzakhala osakhulupilika ? Mofananamo , mukadziŵa kuti zimene Mulungu analosela zinacitikadi , mudzakhulupilila kuti zimene amatiuza ponena za mtsogolo zidzacitikadi . Iye anawacha kuti “ anthu amene ndinawapanga kuti akhale anga , anene za ulemelelo wanga . ” ( Yes . Kumeneko , anakumana ndi mai wina “ wolambila Mulungu ” dzina lake Lidiya , ndipo “ Yehova anatsegula kwambili mtima wake kuti achele khutu ” ku zimene zinali kulankhulidwa . — Machitidwe 16 : 9 - 15 . ( Miy . 27 : 11 ) Acicepele amafunika kukhala olimba mtima kuti apewe mabwenzi oipa ndi kukana zosangalatsa zosayenela . Ganizilani za atumwi . Zimenezo n’zoona , koma naonso amafunikila kuwalimbikitsa , kulalikila nao , ndi kuwaitanako ku zosangulutsa zina . Ngakhale n’conco , mwina mungakhale na nkhawa . Magazini iyi ya Nsanja ya Mlonda , ifotokoza mmene tingapindulile na nkhani ya amuna anayi okwela pa mahosi . ( Aheberi 13 : 5 ) Kukhala pa ubwenzi wolimba ndi Yehova kudzatithandiza kuona dzanja lake pa umoyo wathu . M’malomwake , ionetsa kuti anakangana cifukwa cosiyana maganizo pankhani yotenga Yohane Maliko pa ulendo wawo waumishonale . — Mac . 15 : 36 - 40 . N’cifukwa ciani akulu ena sapatula nthawi kuti aphunzitse abale ena mumpingo ? Woumba amaumba cinthu cokongola poseŵenzetsa dothi . Anali womasuka kuwauza zimene anali kuganiza ndi mmene anali kumvelela . Ndipo anali kumvetsela bwinobwino pamene io anali kumuuza zimene anali kuganiza ndi mmene anali kumvelela . ( Maliko 14 : 36 ) Ganizilani mmene ophunzila a Yesu anamvelela pamene anamva , kapena kudziŵa za pemphelo lake . Conco , inu makolo muzikhulupilila kuti cilango ca Yehova na malangizo ake n’zoyenela olo cikhale covuta kwa inu kucita zimene iye walamula . Tidzakambilanso mmene tingapewele kutengela makhalidwe oipa , pamene tikuthandiza anthu mwauzimu . Koma anacita zambili kuposa pamenepo . Comvetsa cisoni n’cakuti , nditayamba kudwala matenda a msana mu 2004 , ndinasiya upainiya . ( Maliko 6 : 34 ) Ngakhale pamene anthu anali kumunenela zacipongwe , Yesu sanabwezele zacipongwe . — 1 Petulo 2 : 23 . “ Anthu ambili amene agona munthaka adzauka . ” — Danieli 12 : 2 . NKHAWA NA KUSOŴA TULO POFUNA KUTETEZA CUMA “ Wotumikila munthu wina amagona tulo tokoma ngakhale adye zocepa kapena zambili . Oct . Kodi kuimba kumatipatsa mwayi wanji ? ( 1 ) Kodi kukhala munthu wauzimu kumatanthauzanji ? Iye “ amatitonthoza m’masautso athu onse . ” ( 2 Akor . Mneneli Yeremiya analemba kuti : “ Dokowe , mbalame youluka m’mlengalenga , imadziŵa bwino nthawi yake yoikidwilatu . ” Kulimbikitsa mwana kukhala na zolinga zakuthupi kungamusokoneze na kumuononga mwauzimu . Kugwila Nchito ndi Mulungu — Kumabweletsa Cimwemwe , Jan . Koma bwanji ngati munthuyo wasiya kumvela Yehova ndi kuyamba cibwenzi mwakabisila ndi munthu amene satumikila Mulungu ? Ndipo n’cifukwa ciani ? Kodi tingatsatile motani malangizo a pa 1 Akorinto 13 : 5 , 6 ? N’nali kucita cidwi na maluso awo pokamba nkhani ndi pofotokoza coonadi ca m’Baibo . M’Baibulo timaŵelenga kuti : “ Ine Yehova ndine Mulungu wanu , amene ndimakuphunzitsani kuti zinthu zikuyendeleni bwino . ” Nyumba yathu yokongola imeneyi inamangidwa m’masiku 8 cabe . Tingalembe malemba amenewa penapake ndiponso tingasunge magazini amenewa kuti tiziwaŵelenga nthawi ndi nthawi . Kucokela pa umwana wanga ndinali ndisanawonetsedwepo cikondi cotelo ngakhale ndi anthu a m’banja langa . Ndipo cofunika maningi kuti tipeze mtendele wokhalitsa ni kukhala pa ubwenzi wolimba na Mulungu . Ana anati : “ Mtendele wa mumtima wocokela kwa Mulungu unakhazika maganizo anga pansi . OSADZIIMBA MLANDU . Yehova anabwela ndi miyandamiyanda ya oyela ake , kudzapeleka ciweluzo kwa onse , ndi kudzagamula kuti onse osaopa Mulungu apezeka ndi mlandu cifukwa ca nchito zawo zonyoza Mulungu zimene anazicita mosaopa Mulungu , komanso cifukwa ca zinthu zonse zonyoza koopsa zimene ocimwa osaopa Mulungu anamunenela . ” Timamvela bwanji tikaona zimenezi ? Kodi kudziŵa Mulungu molondola kunam’thandiza bwanji Yobu ? Mogwilizana ndi zimene Yesu anakamba , tingakonde anansi athu , acibale , mabwenzi athu , ndi ena kokha ngati tikonda Mulungu coyamba . Ngati muona kuti kuŵelenga Baibo kucokela kuciyambi mpaka kumapeto n’kocititsa ulesi , mungayambile kuŵelenga nkhani zimene zimakukondweletsani ngako . Komanso , tiyeni tizisangalala cifukwa coika zinthu za Ufumu pamalo oyamba . Cifukwa ca kusintha - sintha kwa zandale , nazonso zinenelo zimene anthu ambili amakamba zimasintha . Ndipo nthawi ina , nkhani ya cakudya na zakumwa inafika povuta kwambili , cifukwa Danieli anakana ‘ kudzidetsa ndi zakudya zabwino za mfumu . ’ — Dan . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Cimene Mulungu wacimanga pamodzi , munthu asacilekanitse ” — Mateyu 19 : 6 . Kenako Samueli anacita zimene anali kuganiza zija . N’cifukwa ciani mungakonde kuti ena aciteko utumiki umenewu ? 20 : 28 - 30 ; 2 Ates . 2 : 3 , 4 ) Ndipo zinali zovuta kudziŵa amene anali kutumikiladi Mulungu pa kacisi wake wauzimu . Mungapeleke zopeleka zanu kupitila ku banki , kapena mungaseŵenzetse makhadi a ku banki . Akristuwo anaona asilikali aciroma akucoka ku Yerusalemu . Olo munthu atawamenya bwanji , sangatulutse madzi . 31 : 1 - 11 ) Ngakhale n’conco , ndi anthu ocepa cabe amene anaona nchito yapamwamba imene Bezaleli ndi Oholiabu anagwila . Nanga n’cifukwa ciani ? Kuti tisaononge makhalidwe athu abwino , tiyenela kupewa kugwilizana ndi anthu ocita zoipa . 3 - 5 . ( a ) N’ciani cimene Petulo anauza Ayuda patsiku la Pentekosite ? Filipi unali umodzi mwa mizinda yaconco . N’nali kukonda baseball kuposa cina ciliconse . Ngati citsulo canyowa cingacite dzimbili . Mlongo Debbie , amene ali ndi ana aŵili , anati : “ Popeza mwamuna wanga anali mkulu , sindinali kucita nsanje ngati akuceza ndi ena mumpingo . Kodi nimalabadila mofulumila malangizo ocokela kwa otiyang’anila ndi kuwacilikiza ? ’ Tonse tifunika kukhala na zolinga zauzimu cifukwa kucita izi kudzatithandiza kukhala atumiki a Yehova olimba mwauzimu . — Mlal . Kuti mumvetsetse zimene mukuŵelenga m’buku , ilo liyenela kukhala la cinenelo cimene mudziŵa . ( Ŵelengani Aefeso 5 : 23 , 24 . ) Mofanana ndi Paulo , timalalikila anthu cifukwa timawakonda na mtima wonse . Kodi mumatengelapo mwai pa makonzedwe acikondi amenewa kuti muŵete ana anu ? Muzikumbukila Amene Ali mu Utumiki Wanthawi Zonse Abale na alongo ambili amadzipeleka kukalalikila ku madela kumene kuli ofalitsa ocepa . Palibe munthu amene ayenela kulemekezedwa cifukwa ca izi . Kodi tonse mumpingo tili na mwayi wolambila Yehova m’njila iti ? Ndinadziŵanso kuti ngakhale nditayembekeza kwa kanthawi ndisanayambe upainiya , makolo anga adzapitilizabe kunditsutsa . Mapemphelo a anthu ena amacokela pansi pa mtima koma a ena sacokela pansi pa mtima . ( Mat . 24 : 38 , 39 ) Olo kuti anthu analibe cidwi , Nowa anapitiliza kulengeza mokhulupilika uthenga wocenjeza umene anapatsidwa . ( Aheberi 12 : 2 , 3 ) Yesu anaika maganizo ake pa madalitso amene anali kudzalandila cifukwa ca kupilila kwake . Iye anakambanso kuti : “ Kutumikila pa Beteli kumafuna kukhala ndi umoyo wosalila zambili , ndipo kucita zimenezi n’kofunika kwambili m’dongosolo lino la zinthu . ” Kodi fanizo la kanjele ka mpilu limatanthauza ciani ? Sitiyenela kukana thandizo iliyonse Koma tsopano tatambasulani dzanja lanu ndi kukhudza zonse zimene ali nazo , ndipo muona , akutukwanani m’maso muli gwa ! ” ( Mateyu 6 : 26 ) Ndi mau amenewa , Yesu analimbikitsa ophunzila ake ndi kuwathandiza kumvetsetsa mfundo yofunika kwambili . Ziphuphu za m’boma zimatanthauza kugwilitsila nchito udindo umene munthu ali nao m’boma kuti adzipindulitse . A Yohane : Zikomo . 20 : 29 ) Conco , ni njila yacikondi komanso yothandiza kuti acikulile azikonzekeletsa acinyamata kutenga maudindo aakulu . — Ŵelengani Salimo 71 : 18 . 6 : 10 ) Yehova amayamikila zimene timacita kuti timukondweletse , ndipo utumiki wathu sudzapita pacabe . Koma ici sicinali cifuno ca Mulungu poyamba . 18 : 35 ) Conco , kuyenda modzicepetsa ndi Mulungu , kudzatithandiza kusadziganizila modzithuvula , kapena kudzitsitsa modzigwetselatu . — Ŵelengani Aroma 12 : 3 . Nzelu zimenezo zidzatithandiza kuti tisapunthwe mwauzimu . Yehova adzaona kuti kuukila atumiki ake kuli ngati kuukila iye mwini . Makolo , mumafuna kuti ana anu azikhalabe paubwenzi ndi Yehova . Komanso Neko anali kupita kukacita nkhondo ku Karikemisi . Iye anali kupita kukamenyana “ ndi mtundu wina , ” osati Yerusalemu . Gwen : Yehova anatithandiza kupilila mavutowo . Koma kodi timacita bwanji tikakumana ndi mavuto ena ooneka ngati ang’ono - ang’ono ? Iye anali atangotumiza ophunzila ake 70 kukalalikila uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . Koma kodi cinacitika n’ciani pambuyo pake ? Zinthu izi zilibe vuto pa izo zokha , ni mbali ya umoyo wa munthu . Munthu amene ananyamula kacikwama konyamulilamo inki aimila Yesu Khiristu . Baibo imacenjeza kuti amene aloŵa m’banja “ adzakhala ndi nsautso m’thupi mwawo . ” ( Aef . 1 : 7 ) Ngati pali umboni waukulu umene Mulungu anapeleka woonetsa mmene amatikondela , ni nsembe ya dipo ya Khiristu . Ndakhala wozindikila kwambili kuposa aphunzitsi anga , cifukwa ndimasinkhasinkha zikumbutso zanu . Mulungu angauseŵenzetse kutonthoza aliyense amene ali na vuto lililonse . Iye anayang’anitsitsa dzanja lamanja la Atate , kuonetsa kuti anali kufuna kubatizika . Anadziŵanso kuti anafunika kucita nchito yaikulu asanaphedwe . Iye anali wokonzeka kupita . ( b ) Mungadziŵe bwanji thandizo limene mwana wanu afunikila ? Mkazi wanga nayenso anali mpainiya , ndipo anali kucilikiza atsikanawo masiku onse . “ Kuti tipeze moyo kudzela mwa iye . ” Pa cifukwa cimeneci , ndinayamba kuwakonda kwambili , ndipo ndinali kudzimva kukhala wokhutila ndiponso wotetezeka . ” Nditakhutila ndi mayankho a m’Baibulo amene anandiuza , ndinavomela kuphunzila Baibulo . ” — Gill , England . Ofufuza zinthu zakale anapeza cikalata cimene cinachulako za “ nyumba ya Davide . ” Monga mmene n’nali kucitila kale , anzanga ku nchito anali kutumizilana zithunzi - thunzi zimenezi . Onani nkhani yakuti , “ Kodi N’zotheka Kuyamba Kukhulupilila Mlengi ? ” ( Mac . 20 : 28 , 29 ) Kumbukilani kuti ndi udindo wanu kuphunzitsa , kulimbikitsa , ndi kutsitsimula nkhosa zake . ( Yes . Nkhani zolembedwa za m’nthawi imeneyo zionetsa kuti munthu anali kugulitsidwa ndi kupita ku ukapolo ku Iguputo ndi masekeli 20 . [ Cithunzi papeji 10 , 11 ] 38 : 8 - 12 ) Pa nthawiyo , tidzakhala wokondwa kwambili podziŵa kuti tinayesetsa kukhala wodziŵika kwa Mulungu osati ku dzikoli . Iye anadandaula kuti : “ Mwamuna wanga atapita kunchito sanabwelelenso kunyumba , ndipo iye anali ndi zaka 52 cabe . ” Panthawiyo , nchito yathu yatsopano idzakhala yokonza dziko lapansi kuti likhale paladaiso . 10 : 6 ; 15 : 24 ; Luka 19 : 10 ) Pacifukwa cimeneci , Yesu analalikila mwacangu za Ufumu wa Mulungu . Cifukwa ca kukoma mtima kwake kwakukulu , Yehova anatipatsa mwayi wokamba naye m’pemphelo . Mwacitsanzo , nkhani ya pamsonkhano wa cigawo mu 1958 inali ndi mutu wakuti : “ Ufumu wa Mulungu Ulamulila — Kodi Mapeto a Dziko Ayandikila ? ” Kuti mudziŵe zambili zokhudza Baibulo , onani kabuku kakuti Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani ? ( Aheberi 5 : 14 ) Mkristu wokhwima mwakuuzimu amadziŵa coyenela ndipo amakhala wotsimikiza mumtima mwake kucicita . Iye anati : “ Mwendo wanga wa kumanzele ni waufupi na masentimita 9 kuyelekezela na unzake . Davide anadziŵa kuti Mulungu ndiye anamuthandiza . N’cifukwa n’ciani mfundo imeneyi ndi yovuta kumvetsa ? N’napita patsogolo mwamsanga cifukwa n’nadziŵa kuti napeza coonadi . Panthawiyi ife tinali kukhala pakati pa Europe ndi dziko la London . Malo amenewa panali kudutsa ndeke za nkhondo . 12 , 13 . ( a ) Kodi Yesu anacita ciani cimene cinacititsa cidwi anthu Acigiriki ku Yerusalemu ? YESU KRISTU , Mwana wa Yehova , anati : “ Ndimakonda Atate . ” ( Yoh . Nikhulupilila kuti ngati munthu amavomeleza utumiki uliwonse umene wapatsidwa ngakhale umene saukonda , Yehova nthawi zonse amamudalitsa . Kodi tingagwilitsile nchito bwanji mafanizo pophunzitsa ena ? Nthawi zina limatanthauza thupi lathu leni - leni . N’nali kukondanso nyimbo ndi kuvina . Cina cimene Yesu anacita atabwela padziko lapansi ndi ‘ kulengeza uthenga wabwino wa ufumu wa Mulungu . ’ Nyimbo ya Debora ikuonetsa kuti Sisera anali kubwela ndi akazi ambili kucokela kunkhondo ndipo nthawi zina anali kubweletsela m’silikali aliyense akazi aŵili kapena atatu . Oweruza macaputa 4 ndi 5 , aonetsa kuti Yehova amayamikila ngati ticita modzipeleka zimene iye watilamula . Inde anali nawo , ndipo abalewo atadziŵa , mitima yawo inakhala pansi . 10 , 11 . ( a ) Ni mbali ziti zimene tingafunike kugonjetsa kuti tipeze madalitso a Mulungu ? Anavomelanso pempho langa , koma sanasinthe malipilo anga . ( Malaki 3 : 6 ) Wamasalimo anauzilidwa kulemba kuti : “ Olungama adzalandila dziko lapansi , ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya . ” — Salimo 37 : 29 . Anagwilitsilanso maluso ake na nzelu zake pa nchito imene Mulungu anam’patsa , yomanga cingalawa . — Ŵelengani Aheberi 11 : 7 . Koma io anali kufuna kuonjezelanso utumiki wao . Kapena angayambe kukhala na umoyo wosalila zambili n’colinga cakuti acite zambili potumikila Yehova . Kodi makolo angathandize bwanji ana kukhala ndi cikhulupililo cawo - cawo ? TIKUKHALA m’nthawi yapadela kwambili . Koma tifunika kuika patsogolo cikondi cathu pa Mulungu na Khristu . ( Mat . Yuichiro anapitiliza kunena kuti : “ Ndinaganizanso zoyamba kupanga zosankha zimene zidzandithandiza kutumikila Yehova kumaiko ena mtsogolo . M’dziko loipali , akazi amacitilidwa zinthu zoipa monga kupanda cilungamo , ciwawa , ndi nkhanza . Lemba la Yesaya 65 : 11 linandithandiza kudziŵa mmene Yehova amaonela anthu amene ‘ amayalila tebulo mulungu wa Mwayi . ’ Conco , ulosi umenewu umatipatsa mwayi wodziŵa zimene zinacitika kumwamba . Ofalitsa ndi apainiya anakwanitsa mlingo wa maola 1 miliyoni mu 1938 . N’ciani cingatithandize kuti tizipanga zosankha zabwino ? Munthu ameneyo angakhale kuti nayenso ni wamanyazi ngati ine . ” N’naphunzila zambili kumeneko . Ngati zotelozo zakucitikilani , kodi mungacite ciani ? Nanga n’cifukwa ciani Mose “ anayang’anitsitsa pamphoto imene adzalandile ” ? Anadzipeleka ku Micronesia , 7 / 15 MBILI : ANALI WOLOŴELELA M’ZAMASEŴELA NA NJUGA CAKA COBADWA : 1954 Amakhala na cikhulupililo pambuyo podziŵa Mulungu molondola , kudziŵa cifunilo cake , na njila imene wakonza yopulumutsila anthu . Mkhristu wokhwima mwauzimu amaganizila cikumbumtima ca ena ( Onani palagilafu 11 , 12 ) Titafika m’dziko lokongola limeneli , limene lili kum’mwela cakum’maŵa kwa Asia , tinaona ndi kumva zinthu zosiyana kwambili ndi zimene tinazoloŵela ndiponso tinali kudya zakudya zacilendo . 30 : 12 . ( Ŵelengani Genesis 6 : 5 , 6 ) N’zoonekelatu kuti Yehova safuna kuti tiziganizila za ciwelewele . Salimo 40 : 8 imatiuza mmene iye anali kumvelela . Lembali limati : “ Ndimakondwela ndi kucita cifunilo canu , inu Mulungu wanga . ” Sitifunika kuŵelenga ngati ana a sukulu , amene amangoloŵeza mfundo zinazake kuti akaphase mayeso . A Inoki : Munthu wina wochulidwa m’Baibulo amene anthu anali kutsutsa zakuti analiko ndi Pontiyo Pilato , bwanamkubwa amene anakhalako m’nthawi ya Yesu . ( Ezek . 1 : 1 ; 8 : 1 ) Ayuda osamvela a ku Yerusalemu anali pafupi kuwonongedwa , ndipo anawonongedwadi mu 607 B.C.E . Kodi nkhani ino yakulimbikitsani bwanji ? Pakuti uwu ndi uthenga umene munamva kuyambila pa ciyambi , kuti tizikondana . ” Cikhulupililo ca Mkristu cingayesedwenso ndi matenda osatha , imfa ya mwana wake , kapena mnzake wam’cikwati , kapenanso wacibale wake akasiya kutumikila Yehova . Kuti mupeze mayankho ake , tikupemphani kuti , Koma sitiyenela kuiŵala malangizo a m’Baibulo akuti : “ Munthu amene sadziŵa zinthu amakhulupilila mau alionse , koma wocenjela amaganizila za mmene akuyendela . ” — Miyambo 14 : 15 . Tingacite ciani kuti tiziona nchito yakuthupi moyenela ? Njila imodzi imene timapezela nzelu zocokela kwa Mulungu ni mwa kulandila cilango cake . Tiyeni tikambilane zitsanzo zitatu zimene tiyenela kutengela — ca Yehova , Yesu , na mtumwi Paulo . Iwo anali kuimbila pamodzi nyimbo zosangalatsa zotamanda Yehova m’kacisi . Mafunso a mwana wanu ni umboni wakuti amafuna kuti mudziŵe , kuti mum’thandize kumvetsetsa zinthu . PAMENE izi zinali kucitika , n’nali n’takhala kale na cidwi ndi coonadi ca m’Baibo . Na ise tingatsitsimule ena mwa kukhala aubwenzi na okoma mtima . Mwa ici , tidzalimbikitsa mgwilizano pakati pa abale na alongo mumpingo . Conco , m’madzulo tsiku limenelo n’nayendadi . Koma pambuyo pake anayamba kuphunzila Baibo . Poyamba anacita izi kuti atsimikize mwamuna wake kuti zimene anayamba kukhulupilila n’zabodza ! 1 : 3 - 5 , 7 ; 1 Ates . 1 : 2 , 3 ) Iye anayamikilanso Yehova pa zonse zimene abale ake anam’citila atakumana ndi mavuto . ( Mac . “ Davide anakwanilitsa cifunilo ca Mulungu mu nthawi ya m’badwo wake , ndipo anagona mu imfa . ” — Machitidwe 13 : 36 . Iye angakuthandizeni kupitila m’mau a anthu ena ndi thandizo lawo . * Mwina mungakhale pakati pa abale ndi alongo , acicepele ndi acikulile , okwatila kapena osakwatiwa , amene adzipeleka mofunitsitsa kuti alaŵe cimwemwe ‘ cokolola zoculuka . ’ Kodi dzina lake tingalidziŵe bwanji ? Ena amapanga makonzedwe kuti aonjezele utumiki wao pa nyengo ya Cikumbutso . Mlongo wina wa ku Austria anazindikila kuti Mulungu anaona nchito imene iye anagwila mwakhama . Tinalembelana makalata kwa kanthawi ndithu , ndipo pothela pake tinamanga banja . Kodi mungathe kumukhululukila ? Iye anakamba kuti amacita cidwi ndi mmene mabuku a m’Baibulo amagwilizanilana , ndipo amatha kuona m’maganizo mwake zimene akuŵelenga . Anakambanso kuti : “ Masiku ano ndimasangalala kwambili kuŵelenga Baibulo kuposa kale . ” Ngakhale pano ndimavutikabe maganizo ndikaganizila mmene anthu amandionela limodzi ndi ana anga . Mau amenewa alibenso macaputala ndi mavesi amene ali m’Baibulo masiku ano . N’zoona kuti mwamuna na mkazi amakhala na cimwemwe podziŵa kuti adzakhala na mwana . M’malomwake , nimadzifunsa kuti : ‘ Kodi zokumana nazo mu umoyo wawo zakhudza bwanji maganizo awo na mmene amamvelela ? N’ciani cinacititsa kuti Mose ayambe kukonda Yehova ? Kodi tidzapindula bwanji ngati tiyesetsa kukonza cipulumutso cathu ? Yehova ndiye mwini golide na siliva yense , kuphatikizapo zinthu zina zonse zacilengedwe . Zinthu zimenezi amaziseŵenzetsa pocilikiza zamoyo . ( Sal . Kodi malo amenewa analikodi ? ( b ) Ndani amapindula pamene tithandiza ofooka ? SIKUONONGEDWA KWA DZIKO NDI MOTO . Kuti mudziŵe zambili , onani nkhani 17 m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , yofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . ( Yes . 55 : 7 ) Tikacita zimenezi , iyenso adzakhala ku mbali yathu mwa kutilimbikitsa na kutipatsa mphamvu zimene zingatithandize ‘ kugonjetsa ’ zilakolako zathu za ucimo . — Gen . 12 : 12 , 13 . Federico anati : “ Antonio ananimvela cisoni . Akhristu ena amaona kuti sangakwanitse kuceleza alendo cifukwa kaŵilikaŵili amakhala otangwanika na olema . ; ndipo muziseŵenzetsa zida zimene muli nazo kuti mufufuze mfundo zowonjezela pa zimene mwaŵelenga . — w16.05 , mapeji 24 - 26 . Kenako , iye anadabwa kwambili kuona kuti acicepele onse akupatsidwa buku lakuti : Achichepere Akufunsa — Mayankho Amene Amathandiza . Iwo amayendela limodzi ndi abale a m’Bungwe Lolamulila ku misonkhano yapadela ndi ya maiko . Iwo anadabwa kwambili , ndipo anandifunsa kuti , “ Ndi pati makamaka m’Baibulo ? ” “ Mapeto a nthawi ino ” anayamba mu 1914 . Koma kampasi yoseŵenza bwino ingathandize woyendetsa kudziŵa kumene afunika kuloŵela . M’nkhani yapita , tinakambilana za Kaini , Solomo , ndi Aisiraeli . Ndithudi , nchito za Nowa zoonetsa cikhulupililo zinacititsa kuti iye na banja lake apulumuke Cigumula . Pa zandale , Afarisi anali kufuna kuti Ayuda akhale na ufulu wodzilamulila okha . Kuti acite zimenezi , ambili amasiya mabanja ao ndi kupita ku dela lina la m’dziko lao kapena kupita ku dziko lina . Iye anawalimbikitsa kuika maganizo ao pa kutumikila Yehova , ndi kuika Ufumu wake pamalo oyamba . Aisraeli anali kudziŵa “ mmene zimakhalila ukakhala mlendo . ” Ndine wokondwa kuti ambili acitadi zimenezo . ” Tifunika Kukhala Oyela m’Makhalidwe Athu Onse ( Luka 4 : 16 , 17 ; Machitidwe 17 : 11 ) Kodi mipukutu yakale imeneyo inapulumuka bwanji ? Yaeli anaona mmene Akanani anali kupondelezela anthu ndipo iye anafunika kusankha cocita . Ndiye cifukwa cake buku la Chivumbulutso limasonyeza kuti Satana ndiye wakhala akucititsa mavuto padziko lapansi kuyambila mu 1914 . Anthu amenewo anali kukhulupilila kuti milungu yawo ingalamulile zinthu zina zacilengedwe . Mogwilizana ndi Danieli 4 : 17 , ulosiwo unapelekedwa “ ndi colinga cakuti anthu adziŵe kuti Wam’mwambamwamba ndiye woyenela kulamulila maufumu a anthu , ndiponso adziŵe kuti iye akafuna kupeleka ulamulilo kwa munthu aliyense amamupatsa . ” Kale , atumiki a Mulungu anali kulalikila uthenga wabwino kwa anthu okhala m’madela akutali pogwilitsila nchito wailesi . Ni mmenenso zilili pa umoyo wathu wauzimu . CINANSO CIMENE MUNGACITE : Mukamvela nkhani ina yake imene yangocitika kumene , pezelamponi mwayi wophunzitsa ana anu mfundo za makhalidwe abwino . Nditakwanitsa zaka 28 , ndinakwatila . Kucita zimenezi sikunali kopepuka , koma abale ndi alongo amenewa anadzipeleka ndi mtima wonse cifukwa cokonda Yehova ndi anthu . 10 , 11 . ( a ) Kodi citsanzo ca Sauli cionetsa bwanji kuti kukhalabe ndi mzimu wodzimana n’kofunika ? Mofanana ndi banja limeneli , anthu ambili angadabwe ndi kuona mtima kwa Haykanush ndi mwamuna wake . Kucita zimenezi kudzakuthandizani kuyembekeza Yehova kuti akupatseni thandizo lofunika . Muziwauza mfundo zanu za makhalidwe abwino . M’kupita kwa nthawi , maudindo ena atsopano anan’thandiza kusinthanso m’mbali zina . 18 : 21 , 22 ) Apa Yesu anali kutanthauza kuti palibe malile a nthawi imene Mkristu angakhululukile ena . — Miy . 10 : 12 . * Poona kuti Marita anali ndi zocita zambili , Yesu mokoma mtima anamuuza kuti : “ Marita , Marita , ukuda nkhawa ndiponso kutanganidwa ndi zinthu zambili . ” ( Luka 11 : 10 - 13 ) Izi zitifikitsa pa njila yacitatu yocepetsela nkhawa zanu — cipatso ca mzimu . Koma Yehova sanaleke kulamulila . Ubwino Wotsatila Malangizo a Yehova ( zocitika mu utumiki ) , Sept . ▪ Kodi Mukuyesetsa Kufika pa Ucikulile Umene Kristu Anafikapo ? Ndiyeno Maxine anayamba kuyang’anila ndalama zimene anthu anali kulipila kuti alandile magazini . 7 : 12 ) Kodi tingatsatile bwanji malangizo amenewa ? Inunso lingakuthandizeni . Abulahamu anapatsa mtumiki wakeyu udindo waukulu wopita ku Harana , kwa acibale a Abulahamu kuti akatengele Isaki mkazi . — Genesis 24 : 34 - 38 . Mmene Akulu Angathandizile Ena Kukhala Oyenelela Maudindo N’taphunzila Baibo , n’nazindikila kuti nifunika kusintha zina na zina paumoyo wanga kuti nikhale na makhalidwe abwino amene Mulungu afuna . ( Aroma 9 : 1 - 3 ) N’cifukwa ciani Paulo anamvela conco ? Kuganizila zovuta zimene munthu wopha mnzake anali kukumana nazo , kunathandiza Aisiraeli onse kuona kuti moyo wa munthu ni wopatulika . Cifukwa ca dipo , timatumikila Mulungu tili na cikumbumtima coyela ndipo timapeza cimwemwe ceni - ceni pocita zimenezi . — Sal . Ndiponso muyenela kuona umenewu ngati mwai wolimbitsa ubwenzi wanu ndi Yehova . Zimene abale ake anam’citila zinamuŵaŵa kwambili . Hana , mtumiki wokhulupilika wakale wa Mulungu , anali kufunitsitsa kukhala na mwana . ( Ekisodo 23 : 8 ) Kucita ziphuphu sikutanthauza kulandila cabe ndalama kuti munthu umucitile cinacake . Kodi Yehova anamva bwanji pamene anaona mmene mtumiki wake wokhulupilika anavutikila ? Tikamatengela Yesu , timakula ndi kukhala Akristu ofikapo kuuzimu , timayandikila Yehova kwambili , ndipo timakhala ofunitsitsa kum’tumikila . Iwo anaona kuti Yehova anawathandiza kwambili panthawi ya cigumula ca madzi cochedwa tsunami cimene cinacitika mu 2011 ku Japan . Mwacitsanzo , kumbukilani pamene munapatula nthawi kuthandiza munthu wokalamba . Posankha zovala , atumiki a Mulungu amazindikila mfundo yakuti pali “ nthawi yocitila cinthu ciliconse ndiponso yokhudza nchito iliyonse . ” Munthu woika maganizo ake pa zinthu za thupi amasumika maganizo na mtima wake pa zolakalaka ndi zofuna za thupi lake lopanda ungwilo . Amangokhalila kukamba mokokomeza zinthu za thupi . * Yesu anawayankha kuti : “ Ana a m’nthawi ino amakwatila ndi kukwatiwa . Koma amene ayesedwa oyenelela kudzapeza moyo pa nthawi imeneyo ndi kudzaukitsidwa kwa akufa sadzakwatila kapena kukwatiwa . Kodi cidziŵitsoco cifunika kukhala coculuka bwanji ? 1 : 16 ) Pambuyo pakenso , Yesu anapatsidwa mbali ina pano padziko lapansi . Coyamba anabadwa monga khanda , ndipo anakula . ( Afil . Tizithandiza anthu mwakuuzimu . Zina mwa zinthu zimenezi si zoipa iyai , koma zinthuzo zingatidyele nthawi yathu . Ponena za mkate iye anati : “ Mkate uwu ukuimila thupi langa . ” Timaŵelenga za Mfumu Davide , mneneli Eliya ndi mtumwi Paulo . Kodi wokamba nkhani angacite ciani kuti Malemba akhale maziko a nkhani yake ? Cifukwa ca dyela , Adamu ndi Hava anapandukila Mulungu amene anawapatsa moyo ndi zonse zimene anali nazo . Koma akalibe kuyenda ku Tennessee , atsikana athu anapanga ulendo wokaceza ku Beteli ya ku London m’dziko la England . Kodi lakhalapo kwa zaka zingati ? Mofanana ndi Rute , Akhiristu padziko lonse lapansi sakaikila zakuti Yehova adzawathandiza . Kodi Akristu ena anapita kukamuthandiza ? Tetragalamatoni : Mmene dzina la Mulungu anali kulilembela m’Ciheberi coyambilila . Ngati mufuna kudzagwila yabwino ya oyang’anila acikristu mtsogolo , yesetsani kukalamila mwa kuthandiza mpingo kukhala wacimwemwe . Mungacite Ciani Kuti Muzisangalala Ngati Mumagwila Nchito Yolimba ? 4 Zoonadi , Ambuye Yesu anapatsa Paulo thandizo lofunikila . Koma ine sinikwanitsa cifukwa nilibe manja . Palipano , tingati Mulungu akuwakumbukila , kufikila “ pamene onse ali m’manda acikumbutso . . . adzatuluka . ” ( 2 Mbiri 14 : 8 - 10 ) Kodi mungacite bwanji mukaona gulu lalikulu limenelo likuloŵa mu ufumu wanu ? Kucotsa wolakwa mumpingo kumacititsa kuti dzina la Yehova lilemekezedwe . “ Munthu wobadwa kwa mkazi , Amakhala ndi moyo waufupi , wodzaza ndi masautso . 2 : 9 . Cikondi pa Mulungu cikukulila - kulila pakati pa anthu ake . Ndipo caka ciliconse , anthu ambili amabwela m’gulu lathu . Koma tiyeni tiimebe zolimba ku mbali yake , cifukwa ‘ Yehova Mulungu wathu ’ ndi amene tiyenela ‘ kumuopa , kum’tumikila , ndi kum’mamatila ’ ! — Deut . Tiyenela kukumbukila mfundo ziŵili zofunika kwambili . Sinidzaiŵala zimenezo . ” Mu 2004 , Cathy ali ndi zaka 31 , anasamukila ku Taiwan , ndipo iye wakhala ndi umoyo wosafuna zambili . 6 : 9 , 10 ) Tidzasangalalanso kwambili kuona colinga ca Yehova cakuti anthu adzadze dziko lapansi cikukwanilitsidwa . ( 1 Akor . 15 : 33 ) Tikawalandila bwino mumpingo , ndiye kuti tikugwila nchito na Yehova yoyang’anila kapena kuti kuteteza alendo ocokela m’dziko lina . — Sal . Mwacitsanzo , pamene mtumwi Yakobo ndi Yohane anafuna kuti akakhale pa malo apamwamba pamodzi ndi Yesu mu Ufumu wa Mulungu , Petulo anakwiya kwambili . 16 : 3 . Ena anganene kuti anadzipeleka kale kwa Yehova koma si okonzeka kubatizidwa . M’nkhani yoyamba , tidzaona zimene munthu amene wacita chimo masiku ano angacite kuti athaŵile kwa Yehova . 11 , 12 . ( a ) Kodi citundu cingakhudze bwanji mmene mwana amapindulila na misonkhano ? Anthu ena masiku ano amacita zabwino ndi kudana ndi zinthu zoipa ngakhale kuti sadziŵa miyezo ya m’Baibulo . Hana 15 : 23 ) Conco , sitiyenela kukayikila kuti kuuka kwa anthu okhala padziko lapansi , nakonso kudzacitika mwadongosolo . Caciŵili , Yehova anam’dzoza monga Mfumu ndiponso monga Mkulu wa Ansembe . ( Sal . Ayuda ambili anali kuyembekezela kuti Mesiya adzacotsa ulamulilo wa Aroma na kubwezeletsa ufulu kwa Aisiraeli . Pomalizila pake , ndinapempha kuti ndikambe ndi wansembe . Ndinamuuza zonse zimene zinacitika . Khalani Maso ! Satana Akufuna Kukumezani Anthu amene amagwilila nchito pamodzi , kaŵili - kaŵili amakhala pa ubwenzi wolimba . Komabe , colinga copelekela malangizo amenewa si cakuti likhale lamulo limene mipingo iyenela kutsatila . Iye anaphunzila za udokotala . Nanga amaonetsa bwanji kuti akali kuvomeleza kaphunzitsidwe kameneka ? Alendowo anali Mboni ziŵili zimene zinali kubwela kaŵili - kaŵili kunyumba kwawo . ( Ŵelengani Genesis 4 : 3 - 7 . ) Panthawi imene munali kufuna thandizo , kodi mmodzi wa atumiki ake , monga mkulu kapena Mkristu wokhwima anakuthandizamponi ? ( Agal . Tsopano , ndine wokondwa kugaŵanamo pa nchito yokonza cakudya ca kuuzimu ndi kucigaŵila kwa abale padziko lonse . Mwakutelo , ‘ amakopedwa ndi kukodwa m’cilakolako cao . ’ Ndiyeno cilakolako cikakula , amacita ciwelewele . Ndi Yesu Kristu woukitsidwayo . — Chiv . * Bukuli linakonzedwa kuti lithandize anthu kumvetsa ziphunzitso zoyambilila za m’Baibulo . Komabe , patangopita miyezi 6 , zinthu zinasintha . Tingapindulenso pamene tipezeka pamisonkhano yacikristu , kumvetsela mosamala , kupeleka ndemanga , ndi kusinkhasinkha zimene taphunzila . ( b ) Nanga n’ciani cinacitika pamene akazi anafika kumanda ? Lembani kalata pogwilitsila nchito keyala imene ili pa tsamba 2 la magazini ino . Zaka zambuyomu makolo anali kudela nkhawa kuti mwina mwana wao amasuta fodya , amamwa moŵa kapena kuvina monyanyula . Koma masiku ano timamva malipoti oipa kwambili . Ŵelengani Mateyu 25 : 14 - 30 . Iye anati : “ Podziŵa kuti ku Russia ndi kozizila kwambili ndinayamba ndayesa kukhala m’dzikolo kwa miyezi 6 ndipo ndinapita mu November n’colinga cakuti ndione ngati ndingakwanitse . ” Kodi maiko aphunzilapo kanthu pa zimenezi , na kuleka nkhondo ? Melissa na a m’banja lake atakukila mu mpingo wina , anali kucita zinthu zowathandiza kupeza mabwenzi atsopano . Pulofesa Martin Goodman , wa pa Univesite ya Oxford , anakamba kuti : “ Kumayambililo kwa ulamulilo wa Roma , nchito yolalikila inasiyanitsa Akristu ndi magulu ena a zipembedzo , kuphatikizapo Ayuda . ” Zimatithandiza kukhalabe bwenzi lake ndiponso kukhala ndi cikhulupililo colimba . — Tito 2 : 2 . Kodi kudziŵa coonadi ponena za Yehova na mfundo zake kumatithandiza bwanji kusankha anzathu abwino na zosangalatsa zoyenela ? Mwacionekele , zipatso zimenezi zimatanthauza nchito imene aliyense wa ise angakwanitse kucita . Motelo Yehova anadalitsa Elisa cifukwa ca kukhulupilika kwake mwa kumulola kuona zimene zinacitika pamene Eliya anatengedwa modabwitsa . — 2 Maf . Mlongo wina wazaka za m’ma 80 anati : “ Ndaŵelengapo buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu nthawi zambili , koma kalembedwe aka ndiponso mmene tumitu twa nkhani tunalembedwela zandithandiza kumvetsetsa kwambili ulaliki wa pa phili . ” Iwo ayenela kukhala odekha kaya ali kale paudindo kapena ai . M’madela ena , amuna sakhala omasuka kuimba pagulu . Ngakhale lomba , siningakwanitse kufotokoza kukula kwa cisoni cimene tinali naco . ( Aheberi 5 : 14 ) Kodi mukukumbukila nthawi inayake pamene simunagonje pa ciyeso kapena pamene munakana kutengela zocita za anzanu ? ( Yesaya 48 : 17 , 18 ) Mwacitsanzo , Baibo ingakuthandizeni ( 1 ) kupanga zosankha mwanzelu , ( 2 ) kupeza anzanu eni - eni , ( 3 ) kucepetsa nkhawa , komanso ( 4 ) koposa zonse , kudziŵa zoona ponena za Mulungu . Utumiki wathu umathandiza kutsutsa mabodza a Satana ponena za Yehova . — Yes . Kuciyambi kwa zaka za m’ma 1920 , Yehova anathandiza anthu ake kumvetsa fanizo limeneli . Mu 2012 , bungwe lofufuza nkhani la Pew Research Center , linapeza kuti ku United States , 11 pelesenti ya anthu amene sakhulupilila kuti kuli Mulungu , amapemphela kamodzi pa mwezi . ( b ) Yehova anacita ciani ndi apandu amenewo patapita zaka mahandiledi ? Komabe , iye anakambanso kuti : “ Koma mwa kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu , ndili monga ndililimu . ” ( 1 Akor . Koma , Sukulu ya Hillel inakamba kuti mwamuna angathetse cikwati cake mwalamulo ngati ayambana na mkazi wake , ngakhale pa nkhani zing’ono - zing’ono . Koma Yesu anawacenjeza za zimene zingapangitse munthu kucita ciwelewele . Mkuluyu amaona kuti ngati aŵelenga nkhani zimenezo , kuwonjela pa kuŵelenga na kusinkha - sinkha Malemba a pa nyengo ya Cikumbutso , amaphunzila mfundo zatsopano caka ciliconse . ( Mat . 21 : 43 ) Anthu okha amene ali “ m’pangano latsopano , ” malinga ndi zimene Yehova anakambilatu kupyolela mwa mneneli wake Yeremiya , ndiwo amapanga mtundu watsopano , umene ndi Isiraeli wa kuuzimu . Anthu amene amakhalabe ndi maganizo amenewo , amaona mfundo yokhala ndi “ zaka zambili ” kuti ndi loto cabe . Tinakhala m’gulu la othandiza pa nchito yomasulila zofalitsa zathu m’zinenelo zina zoonjezeleka . Munthu wina amene anapita kukaona malo amenewa anakamba kuti : “ Munthu amene anali kutionetsa malo anatipeleka ku Cigwa ca Ela . Iye sanali wacipembedzo . Iye amafuna “ kusonkhanitsanso zinthu zonse pamodzi mwa Khristu . ” Koma anacitapo zolakwa zina zazikulu . Fotokozani mmene tingagwilitsile nchito tumapepala twauthenga kuti tiyambitse maphunzilo a Baibulo . POKAMBA za mmene azibusa a machalichi amavalila pa misonkhano yawo , nyuzipepa ina ya ku Netherlands inati : “ Amavala motailila maka - maka kukakhala kotentha . ” Lauri anamwalila mu 1990 , ndipo nayenso anali wokhulupilika kwa Yehova . Conco , ndi bwino kuti Yehova analola Yona kulemba yekha nkhani yake , kuphatikizapo pemphelo lake kwa Mulungu pamene anali pansi pa nyanja . Kodi tifunika kucita ciani kuti Baibulo itiumbe ? Nthawi zina kungowafotokozela cifukwa cake zinthu zina n’zabwino zina n’zoipa n’kokwanila . Komanso kugwila nchito mwakhama kumathandiza munthu kuti azidziona kuti ndi wofunika . Kodi tiyenela kumva bwanji tikaganizila mphatso yamtengo wapatali imeneyi ? Kodi Rakele anakwanitsa bwanji kucilimika polimbana ndi vuto lalikululi ? Tiyeni tione zimene zinacititsa kuti Yesu akambe mau amenewa . Pamene Mulungu anali kulenga dziko lapansi , angelo anali kuona ndipo anafuula ndi cisangalalo . — Yobu 38 : 4 - 7 . Koma kuti tionetse kuti tili ku mbali ya Yehova , tifunika kukhala omvela nthawi zonse , kwa moyo wathu wonse . — 1 Pet . Pamene Daniel anali na zaka 4 , anadwala matenda oopsa a khansa ya m’magazi . Mwina Samueli anali kudzifunsa kuti , ‘ Kodi munthu ameneyo ndingamuthandize bwanji kukonzekela udindo wake ? ’ Timaona kuti ndi mwayi kukhala m’banja lacikhiristu la pa dziko lonse , limene muli anthu acikondi ndi amakhalidwe abwino . Yesu atatsala pang’ono kuphedwa , zinthu zinali zovuta kwambili pa umoyo wake . 34 : 18 ; Yes . 57 : 15 ) Iye amatipatsa nzelu ndi mphamvu zotithandiza kupilila mavuto aliwonse amene tingakumane nawo . — Yak . ( 1 Timoteyo 2 : 9 ) Pa lembali mau akuti “ zovala zoyenela , ” akutanthauza zaulemu ndi zooneka bwino . N’cifukwa ciani ino ndiyo nthawi yofunika kuonetsa kuti tikucilikiza ulamulilo wa Yehova ? M’malomwake , tengamponi phunzilo , konzani zinthu , na kucita zoyenela . ( Aroma 3 : 23 ) Mwacitsanzo , mkazi asanakwatiwe amafunika kugonjela ulamulilo wa makolo , koma akakwatiwa amafunika kugonjela ulamulilo wa mwamuna wake . Kwa ine , iye ni wamtengo wapatali kuposa mwala uliwonse wa dayamondi , ndipo ndine wokondwa ngako kuti tinakwatilana . Ganizilani cabe za masinthidwe amene acitika pa zaka 10 zapitazo , ndipo musaiŵale kuti Yehova ndiye wacititsa zimenezo . Komabe , si acicepele okha amene amakumana na mavuto . Kenako anaonekela kwa Yakobo , kenakonso kwa atumwi onse . Ndiponso , Mulungu anaonetsa kuti ali ndi mphamvu zokwanilitsa malonjezo ake onse . lonjezo lanu la cikwati ? Pamene tipitiliza kuyenda na Yehova , kudzicepetsa kwathu nakonso kuyenelanso kukulila - kulila . Ganizilani mmene mipukutu ya “ malemba oyela ” imene anali kugwilitsila nchito m’nthawi ya Paulo inali kuonekela . Ndinakhudzidwa kwambili kudziŵa kuti Mulungu ali ndi dzina lake , cinthu cimene cikhalile sindinamvepo . ” Pamene Yesu anakamba za ‘ kubwela ’ kapena kufika kwake , anali kutanthauza za nthawi ya cisautso cacikulu pamene iye adzabwela kudzaweluza ndi kuononga dziko loipali . ( Yuda 14 , 15 ) Mosakayikila , ulosi wa Inoki unathandiza Nowa kukhala na ciyembekezo komanso cikhulupililo colimba . Conco , ndinafuna kum’nyengelela kuti abwelele ku Katolika . N’nalibe nkhawa pa umoyo wanga ndiponso n’nali kukhala wosangalala . M’bale Henschel ananiuza kuti kuyambila nthawiyo udindo wanga waukulu pa Beteli udzakhala kuthandiza M’bale Franz pa zilizonse zimene angafune thandizo . ( Yakobo 1 : 5 ) Tikapempha nzelu kwa Mulungu , iye amatipatsa mzimu woyela kuti utithandize kusankha zinthu mwanzelu . Koma timayamikila kwambili zimene ena amacita potithandiza kucepetsa mavuto athu . Baibo imati : “ Mawu a Mulungu ndi amoyo . ” — Aheberi 4 : 12 . Nanga colinga ca moyo n’ciani ? Pakupha munthu , anthu anali kukhokhomela miyendo ndi manja ake pamtengo ndi misomali . Koma zimenezi ndi nkhambakamwa cabe . Atangokhala Mfumu , iye anayamba nkhondo yolimbana ndi dziko loipali . N’cimodzimodzinso ndi Mulungu , iye amatipempha kuti tizikamba naye n’colinga cakuti tikhale naye paubwenzi wabwino . 3 : 15 ) Alembi na Afarisi anali onyada ndi odzikonda , ndipo sanali kulemekeza moyo kapena kuona ena kukhala ofunika . Anatumiza mwana wake wamkazi namwali ku Silo kuti akatumikile ku cihema kwa moyo wake wonse . — Ower . M’kupita kwa nthawi Paul na Stephany anamanga banja pambuyo pokwanitsa zaka 23 . Panthawi ya misonkhano ya dela ndi ya cigawo , mavalidwe athu ayenela kukhala abwino ndi aulemu . Ngakhale n’conco , ndinafunabe kudziŵa cifukwa cimene anthu amafela ndiponso cifukwa cimene Mulungu walolela kuti azivutika . Anali kulalikila anthu amene anali kudziŵa Mulungu wa Abulahamu , ndipo anali kukamba nawo mwa kuseŵenzetsa Malemba Aciheberi . — Mac . Kuwonjezela apo , Satana anapeleka lonjezo labodza kuti : “ Mudzafanana ndi Mulungu . Kodi Yesu anaonetsanso bwanji kuti anali wozindikila ? Loïs wa zaka 11 ku Togo ananena za mzimu umene banja lao lili nao kuti : “ Ngakhale kuti nthawi zina tingayambe kulambila kwathu mocedwa cifukwa ca zinthu zina zimene zacitika pa tsikulo , timaonetsetsa kuti sitinaphonye . ” Nanga bwanji inu ? Mwina simungafunikile kupita kukakamba ndi wolamulila wamphamvu . NYIMBO : 65 , 48 Ana amafunika kukhala na cikhulupililo colimba , cimene cingawalimbikitse kudzipeleka kwa Yehova mwa kufuna kwawo na kum’tumikila na mtima wonse . Mateyu 24 : 14 : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” Izi ndi zimene walonjeza . * Mu 1996 , tinatumizidwa ku nthambi ya ku Fiji . Kumeneko tinapatsidwanso nchito yothandizila anthu omasulila mabuku m’Cifijiya , Cikiribati , Cinauru , Cirotuma , ndi zinenelo zina za ku Tuvalu . Tsiku lina m’baleyo ananiitana kunyumba kwawo kuti tikamwe tiyi . Conco , pamene Yonatani anafuna kuthandiza Davide , Sauli anakwiya kwambili ndipo anamucititsa manyazi pamaso pa anthu ambili . ( Genesis 16 : 4 - 9 , 16 ) Panthawi imene uthenga wa Yehova unamvekanso , Sara anali na zaka 89 ndipo mwamuna wake anali na zaka 99 . Ndi malangizo otani okhudza cikwati amene Mulungu anapatsa Aisiraeli ? N’kaganizila zimenezi nimakondwela kwambili . Ndipo mudzacita zinthu mozindikila ndi mwanzelu m’dziko loipali . — Miy . Koma anayesetsa kundionetsa cikondi mwa njila imeneyo . Mungamuŵelengele nkhani zimene amakonda kapena kumuimbilako tunyimbo tumene tumam’limbikitsa na kumusangalatsa . N’cifukwa ciani Baibulo silipeleka malangizo acindunji okhudza kusamalila makolo okalamba ? Mlongo wacicepele dzina lake Emily anati : “ Pamene ndikambilana ndi makolo anga za cibwenzi , io sakamba monga kuti ndi nkhani yoipa . Tikamacita mbali yathu , Yehova akutilonjeza kuti ‘ adzamalizitsa kutiphunzitsa . ’ Inde , adzatiphunzitsa khalidwe la kudzicepetsa , ndi makhalidwe enanso aumulungu . — 1 Pet . Kutaca m’maŵa , akulu - akulu a boma anatumiza asilikali kuti akamasule Paulo na Sila ndi kuwauza kuti acoke mumzindawo mwamtendele . Iye anati : “ Ndimatumila foni anzanga amene ndi odwala kapena amene alefulidwa ndi zinthu zina ndipo ndimawalembela makalata . ” Inde , koma tifunika kulimbikila . kukhulupilila pambuyo pokhutila . Iye anagogomeza mfundo yakuti , Akhristu onse odzipeleka afunika kugwila nchito yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu ndi mtima wonse . Iye ananenanso kuti cakudya conse ca m’dzikolo cidzatha cifukwa ca njalayo . — Genesis 41 : 25 - 32 . Mvelani anthu amene amakonda Yehova , amene amakukondani ndiponso amene amadziŵa bwino mikhalidwe yanu . Popeza ndiye Mlengi wathu , amamvetsetsa tikavutika maganizo komanso tikakhala na cisoni . Kumeneko , iye sanaone munthu aliyense akucita zinthu mwacinyengo pofuna kukondweletsa ena . N’cifukwa ciani zimakhala zovuta kuti tate asamalile banja lake ngati akhala kutali ? Nanga tingapindule bwanji tikamaganizila zinthu zosangalatsa zimene Mulungu walonjeza anthu omvela ? Timakhululukila munthu mwa kuiŵalako zimene watilakwila na kusamusungila mkwiyo . Ndiponso muzikhala na mayanjano olimbikitsana ndi abale na alongo anu . 66 : 1 ) Ponena za “ copondapo mapazi ” ake , iye ananenanso kuti : “ Ine ndidzalemekeza malo oikapo mapazi anga . ” ( Yes . Pokhala anthu olengedwa m’cifanizilo ca Mulungu , kodi timakwanitsa kucita ciani ? Mwacionekele , iwo anaona kuti Yesu angakhale mtsogoleli wabwino ngako . Ngakhale kuti dziko lonse lili kale m’manja mwake , Satana akufunabe kugwila anthu ena . ( 1 Yoh . Inu ndi amene muli ndi mau amoyo wosatha . ” 39 : 5 ; 2 Tim . Kodi mpingo umapindula bwanji ngati akulu amaphunzitsa ena ? Umoyo m’dziko lino ndi wodzala ndi zinthu zosokoneza cakuti zimakhala zovuta kupeza nthawi yosinkhasinkha Malemba . CAKA COBADWA : 1948 Iye anamanga nyumba yake pathanthwe cifukwa coganizila mavuto a mtsogolo . M’mabuku atatu amene Yohane analemba muli mfundo za coonadi zofunika kwambili . Ena amakhulupilila kuti . . . nkhawa na kuvutika maganizo ni mbali ya umoyo wa munthu , pamene ena amakhulupilila kuti nkhawa zimakasila m’moyo wina pambuyo pa imfa . N’cifukwa ciani dzina la Mulungu lifunika kupezeka m’Baibulo ? Nthawi zambili , anthu akhungu amamvetsa zinthu m’njila zosiyana ndi anthu amene amaona . Conco , kaya munthuyo anatilakwiladi kapena ayi , tiyenela kukumbukila kuti kukamba zinthu zimene zingaipitse mbili yake sikungathetse vutolo . — w17.04 , peji 21 . Mwacitsanzo , mlongo wina wa ku Australia , amene lomba ni mpainiya anati : “ N’nayamba kuzonda kwambili azungu cifukwa coganizila kwambili zinthu zopanda cilungamo zimene iwo akhala akucitila anthu a mtundu wa Abolijini . Kulephela kupeza thandizo mwamsanga kungacititse zilakolako zoipa kukula ndi kufika pobala chimo . Izi zingakhumudwitse abale athu ndiponso kunyozetsa dzina la Yehova . TSAMBA 23 • NYIMBO : 87 , 50 Banjalo linapatsa Salvatore ndalama ndi kuthandiza iye ndi mkazi wake kupeza nchito . N’cifukwa ciani kudzicepetsa n’kofunikabe ? ( b ) Kodi tidzakambilana mafunso ati m’nkhani ino ? Ndipo a Mboniwo anandiuza kuti Mulungu amandikonda , ndipo ananditsimikizila mwa kundiŵelengela mau a pa 1 Yohane 4 : 8 . Mwamuna na mkazi sayenela kuonetsa ngati kuti amakondana akakhala pagulu , koma akakhala aŵili n’kumanyozana , osakambitsana , kapena kumenyana kumene . Abale na alongo amene ali na umoyo wodzimana , tifunika kumawayamikila . ( Mateyu 5 : 6 ) Ndinali kudabwa kuti munthu angakhale bwanji wodala pamene ali wosoŵa . Ndinakumbukila kuti nthawi ina abusa anakamba kuti wocita zoipa adzapita ku helo . Cimatiŵaŵa kwambili ngati wina aticitila zinthu zopanda cilungamo cabe cifukwa ndife acikhalidwe cosiyana , ndife a fuko lina , kapena cifukwa ca maonekedwe athu . Tikamatelo , timayamba kuwakonda kwambili . Ndipo pamene Yehova aona kusagwilizana kwa anthu padzikoli , amanyadila kuona mgwilizano umene uli pakati pa anthu ake . — Ŵelengani Zefaniya 3 : 17 . ( Aroma 5 : 8 ) Atate wathu wacikondi , Yehova , anapeleka mwana wake dipo kuti atipulumutse ku ucimo ndi imfa . Patapita nthawi , Yehova anafunsa angelo ake za njila yabwino yopusitsila Ahabu kuti apite kunkhondo kumene adzaphedwa . N’cifukwa ciani tifunika kukhululukila ena ? Iye anacita mantha ndi kufuula kuti : “ Kalanga ine Yehova , Ambuye Wamkulu Koposa ! Ndaonana ndi mngelo wa Yehova maso ndi maso . ” ( Ower . ( Sal . 103 : 14 ) Conco , iye sayembekezela kuti tipilila mwa mphamvu zathu zokha , koma pokhala tate wathu , amatithandiza mwacikondi . Nthaka . Pamene ndinali kugwila nchito ya usilikali , pang’onopang’ono tinayamba kusintha boti loonongekalo kuti likhale boti laling’ono la injini . 5 : 19 ) Yesu anatumiwa padziko kuti akatonthoze “ anthu osweka mtima ” ndi “ onse olila . ” Inunso mukhodza kusinkhasinkha zinthu zimenezi . Yehova anakhadzikitsa Ufumu wakumwamba kuti akwanilitse zimenezi . Olamulila a Ufumuwo ndi Yesu ndi a 144,000 ocokela padziko lapansi . Conco tikalakwitsa m’mbali zina , tizipempha Yehova kuti atikhululukile . Muzithandiza anthu mwauzimu . Tikaŵelenga Baibulo tingapeze mfundo zothandiza kuti tilimbane ndi mavuto athu . — 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 . Cofalitsa coyamba kutulutsidwa mu Cituvalu ndi kugaŵilidwa kwa anthu cinali kapepala koitanila anthu ku Cikumbutso . Kodi mungawathandize bwanji anthu othaŵa kwawo amene akukhala m’dela lanu ? Izi zingatheke ngati tipitiliza kukhala ocilimika mwauzimu . Mwinanso pali munthu wina amene akunamizilani zabodza cifukwa cokucitilani nsanje . Baibo imaonetsa kuti ni anthu cabe amene analengewa ‘ ‘ m’cifanizilo ’ ’ ca Mulungu komanso ‘ mofanana ’ naye . ( a ) Kodi ophunzila masiku ano angatsanzile bwanji Elisa ? Mwacitsanzo , yelekezelani kuti mwacita colakwa cinacake cacikulu , ndipo cilango cake ndi kuphedwa . Anailemba ni Wapadela : Baibo ili na mabuku okwana 66 . Amene analemba mabukuwo ni amuna 40 , ndipo anatenga zaka zoposa 1,600 , kuyambila mu 1513 B.C.E . mpaka mu 98 C.E . ( Aheb . 11 : 26 ) Pa lembali , Mose akunenedwa kuti “ Wodzozedwa ” cifukwa cakuti anasankhidwa ndi Yehova kuti atsogolele Aisiraeli kucoka mu Iguputo . cimagwilizanitsa bwanji anthu a Mulungu ? Anafotokozanso kuti unali ufulu wake wolambila ‘ Mulungu wa makolo ake . ’ ( Mac . 5 : 30 ) Ciŵelengelo ca akazi amene anapulumuka Cigumula cinali cofanana ndi ca amuna . Mofananamo , Baibo ili ngati coumba cocititsa cidwi cimeneco . ( Num . 1 : 32 , 33 ) Yosefe analandila madalitso apadela kucokela kwa Yakobo , atate ake . Tili na zimenezi m’maganizo , tiyeni tikambilane ( 1 ) mmene Nowa , Danieli , na Yobu anadziŵila Mulungu , ( 2 ) mmene kudziŵa Mulungu kunawathandizila , ndi ( 3 ) zimene ise tingacite kuti tikhale na cikhulupililo monga cawo . ( b ) Ngati tinacita macimo aakulu koma talapa , tizikhulupilila kuti Yehova adzaticitila ciani ? Motelo mungadzifunse kuti , ‘ N’kangati pamene nkhani zokambiwa pa msonkhano kapena zolembewa m’magazini athu zinanilimbikitsa kusintha maganizo kapena khalidwe langa ? ’ Kodi tingapewe bwanji cizoloŵezi cimeneci ? Zida ndiponso njila zosiyanasiyana zimene takambilana zakhala zothandiza kwambili . Dzifunseni kuti : ‘ Ngati Yesu wabwela ndipo waona zovala zimene ndimavala , kodi ndingacite manyazi ? ’ Yosimbidwa ndi Michiyo Kumagai Koma ndi thandizo la Yehova , n’zotheka kukhala ndi cikwati colimba ndi cacimwemwe . Ndinayamba kumulemekeza kwambili ndi kumuuza mau kuti “ pepani ” ndi akuti “ zikomo . ” Iwo anali kugwilitsila nchito mipukutu . ( Miyambo 14 : 12 ) Koma Yehova amatsogolela bwino kwambili ana ake cifukwa iye ndi “ Mulungu wacoonadi . ” Cikhulupililo ca Inoki ciyenela kutilimbikitsa kudzifufuza kuti tione ngati timaona dzikoli monga mmene Mulungu amalionela . Lemba limene limakamba za cisoni cacikulu cimene Yesu anamvela pamene Lazaro anamwalila , ni lotonthoza kwambili , ndipo n’limodzi cabe mwa malemba ambili - mbili olimbikitsa opezeka m’Mau a Mulungu . 12 : 9 ) Kodi mungacite ciani kuti musasoceletsedwe na mauthenga ake abodza ? Kuti mudziŵe zina zimene mungacite kuti mukulitse luso loimba , tambani pulogilamu ya Cizungu ya JW Broadcasting ya December 2014 ( pitani pa mbali yakuti video , kenako pa FROM OUR STUDIO ) . Lemba la Ezekieli caputala 38 linanenelatu kuti “ Gogi wa kudziko la Magogi ” adzaukila anthu a Mulungu . Kumbali ina , ngakhale kuti timadziona kuti sindife aphunzitsi abwino , tingalalikile mwaluso . Maganizo aconco angakhale amphamvu kwambili cakuti tingakopeke na munthu aliyense amene angationetse cikondi . Ndinapezeka pa msonkhano wa nambala 7 mu August 1951 , ku Austria m’tauni ya Bad Ischl . Ndiponso mu August 1957 , ndipezekanso pa msonkhano wa bungwe limeneli wa nambala 9 ku Sutton Park , pafupi ndi Birmingham , ku England . Njila zosamalila okalamba zimasiyana - siyana . Atamva zimenezi , Sauli anangomuuza kuti : “ Pita , ndipo Yehova akhale nawe . ” — 1 Samueli 17 : 37 . Pewani kukamba zinthu zoipitsa mnzanu wa m’cikwati mukakhala pamodzi ndi ana . Ndiyeno , monga mmene nakambila kuciyambi , wapolisiyo anayamba kuninyengelela kuti nisiye cikhulupililo canga . Tifunikanso kuganizila mmene tingaonetsele kulimba mtima kuti tikwanitse kugwila nchito imene tapatsidwa . M’caputa 6 na 8 ca Aroma , muli malangizo ofunika okhudza umoyo wa ise Akhiristu . 3 : 9 ) Kodi n’zimene inunso mumafuna ? Kukhala wacifundo kudzakulimbikitsani kugwila nchito yolalikila mwakhama , ndipo mwa kucita izi , mudzakhala na cimwemwe coculuka . Kudzikolo , mwapezako anthu ochedwa Afilisiti , zikhalidwe zacilendo monga ‘ kung’amba zovala , ’ cakudya cochedwa mana , ndi ndalama yodziŵika kuti dalakima . Ngakhale kuti mavuto amenewa angaoneke aakulu kwambili , Yehova angatithandize kulimbana nao . N’ciani cinacititsa kuti tipange cosankha cimeneco ? Elisa anaonetsa ulemu kwa Eliya mwa kupitiliza kucita zinthu zimene Eliya anali kucita , ndipo izi zinacititsa kuti aneneli anzake ayambe kum’dalila . Kodi Mkristu aliyense anafunikila kucita ciani kuti akhale wolimba kuuzimu ? Ena amaopa kuti pothela pake adzaluza udindo umene amaukonda kwambili . * Eduardo anati : “ Mwacitsanzo , ndinacotsa ana anga ku masukulu amene si a boma ndi kuwapeleka ku masukulu a boma . ” Ndi nchito yosonkhanitsa iti imene idzayamba Gogi wa Magogi akadzayamba kuukila anthu a Mulungu ? Nanga n’ciani cidzacitika pa nthawi yosonkhanitsa imeneyi ? Ndipo ambili analembedwa m’Cigiriki , conco cigawo cimeneci timacicha Malemba Acigiriki Acikhiristu , cimadziŵikanso kuti Cipangano Catsopano . Komabe , atapempha Yehova kuti awathandize , iye anawapatsa “ mphamvu yoposa yacibadwa , ” ndipo anakwanitsa kuthetsa zizoloŵezi zimenezo . — 2 Akorinto 4 : 7 ; Salimo 37 : 23 , 24 . Iwo anakanidwa ndi kuphedwa . Paulo anaonetsa kuti ngakhale kuti panali Akristu onyenga pakati pao , Yehova anali kuwadziŵa anthu ake monga mmene anawadziŵila m’nthawi ya Mose . 5 : 1 , 2 ) Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Ngati . . . ndilibe cikondi , sindili kanthu . ” ( b ) Ndani amafuna kuononga cikhulupililo cathu ? Kodi zimenezi zingakhudze bwanji cikwati ? Monga anthu okwatilana , io angadzakumane ndi mavuto pa umoyo wao . Koma ngati onse ali pa ubwenzi wabwino ndi Yehova , cikwati cao cidzakhala camtendele ndi cacimwemwe . Atate anakwiya kwambili ndipo anati : “ Ngati uganiza kuti ungapeze nchito , uipeze maŵa , apo ai udzacoka pano pa nyumba . ” Tikagaŵila kapepala kakuti Kodi Zinthu Zidzakhala Bwanji Mtsogolo ? , paulendo wobwelelako tingafunse kuti : “ Kodi Mulungu adzasintha bwanji dziko lathu kuti likhale labwino ? ” Muziganizila mozama zotulukapo za zosankha zanu . Mwamuna ndi kacikwama ka mlembi konyamulilamo inki ndi zolembela ndiponso amuna 6 onyamula zida ( Ezek . 9 : 2 ) , June Ici cinali cizindikilo cakuti anapita patsogolo . Yehova safuna kuti anthu ake aziphunzila Baibulo cifukwa codziimba mlandu . Tingacitenji tikaona kuti tayamba kucita zinthu mosonkhezeledwa ndi kunyada kapena umbombo ? Popemphela nawo pamodzi , iye anakamba kuti anali kufuna kuti ophunzila ake onse akhale amodzi , monga mmene iye na Atate ake alili amodzi . ( Aheb . 5 : 14 ) Malemba ali ndi mfundo zimene zingatithandize posankha zosangulutsa . Yesu ataunika kuti cisudzulo n’cosaloleka kwa Akhiristu oona popanda cifukwa ca cigololo , anakambanso za “ awo ali ndi mphatso ” yokhala ndi umoyo waumbeta . 5 : 19 ) Conco , pokhala Akristu tiyenela kusamala ndi anthu amene timagwilizana nao . Kodi Yesu Anafela Pamtanda ? Tidzakambilana zifukwa zitatu . Ndipo afunikanso kuona kuti cikhulupililo cathu n’colimba . N’cifukwa ciani tifunika kuvala moyenelela ? Polemba , mungagwile mau lemba linalake lolimbikitsa , kuchula khalidwe lina labwino la womwalilayo , kapena kufotokoza zinthu zina zokondweletsa zimene munali kucitila pamodzi ndi womwalilayo . Pamene Yesu anakamba kuti “ mukamasunga mawu anga nthawi zonse , ” anaonetsa kuti pali zinthu zina zimene tifunika kucita kapena malamulo amene tifunika kutsatila kuti iye atimasule . Iye anati : “ Zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inunso muwacitile zomwezo , pakuti n’zimene Cilamulo ndi Zolemba za aneneli zimafuna . ” Matenda amene kale anali kupha munthu mwamsanga apa lomba amatenga zaka zambili . Kodi angamvetsele nyimbo zimene ndimakonda ? Poyankha mau a Ahabu , Eliya anati : “ Inde ndakupezani . ” A Zulu : O - o - o n’zoona . Palibe munthu amene ali na pikica yeni - yeni ya Yesu . Baibo inapangidwa m’njila yakuti anthu odzicepetsa ndi ofunitsitsa kuiphunzila azitha kuimvetsetsa . Mau amene Paulo analembela Timoteyo mouzilidwa amaonetsa kuti iye anali wotsimikiza mtima kuti Mulungu amadziŵa anthu ake . Mu 70 C.E . m’mwezi wa June , Tito analamula asilikali ake kudula mitengo m’dela la Yudeya imene anaiseŵenzetsa kumangila mpanda wa mitengo yosongoka wa makilomita 7 kuzungulila Yerusalemu . Cifukwa cakuti nthawi zambili ana amavutika ndi mabodza a Satana ndi zisonkhezelo za kupanda ungwilo kwao . ( 2 Tim . 2 : 22 ; 1 Yoh . Citsanzo ca mtumwi Paulo cingatithandize kuphunzila kukhala ndi mtima woyamikila . Pamene uthengawu unali kutifika , n’nali n’tayamba kale kudela nkhawa za thanzi la Arthur . Citsanzoci , cikutionetsa mfundo yakuti zosankha zambili zimene timapanga zingalimbitse ubwenzi wathu ndi Yehova kapena kuuononga . Laciŵili lofanana nalo ndi ili , ‘ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ’ ” — Mateyu 22 : 37 - 39 . Abale a ku Turkey amakhala ofunitsitsa kulalikila coonadi kwa anthu ambili mmene angathele . Izi zinamulimbikitsa kulemekeza “ Yehova Mulungu Wam’mwambamwamba , amene anapanga kumwamba ndi dziko lapansi . ” Koma ataipemphelela kwambili nkhaniyo , anasankha kukatumikila ku Wallkill , ndipo amaona kuti anacita bwino . Ndikumbukila nthawi yoyamba imene ndinapita mu ulaliki wa nyumba ndi nyumba . Mukakumana ndi mavuto aakulu mungaone ngati muli pafupi kugwidwa ndi mkango kapena muli kale “ m’kamwa mwa mkango ” monga mmene Paulo anamvelela . NYIMBO : 142 , 92 Patapita nthawi , tinamanga banja . Koma tiyenela kusankha nthawi yabwino yomuuzila zinthuzo kuti apindule kwambili . 7 : 9 , 15 . Ganizilani cimwemwe cimene Timoteyo , Yunike , ndi Loisi anali naco poona kuti Paulo wabwelanso mumzindawo , koma panthawi ino ali pamodzi ndi Sila . Komabe , Charles Taze Russell ndi Ophunzila Baibulo anzake , anapeza cinthu camtengo wapatali kwambili , cimene ndi coonadi ca m’Baibulo . Kodi anthu a Mulungu ali ndi nchito yotani ? Nanga kuti aikwanilitse ayenela kucita ciani ? Kodi Akristu a kumeneko anafunikila kucita ciani ? Imeneyi inali nthawi yovuta kwambili . ” ( Mika 4 : 3 , 4 ) Mabanja acimwemwe “ adzamanga nyumba n’kukhalamo . “ Ndine mmodzi mwa ana 17 . Koma n’zomvetsa cisoni kuti anthu agwilitsila nchito molakwika mphatso yokongola imene Mulungu anatipatsa mpaka afika pakuiononga . Anaonjezela kuti : “ Kwa zaka zonsezi , Yehova wandipatsa cakudya , zovala ndi malo ogona . Kwa ine , zimenezi n’cozizwitsa . ” Yesu adzabwela kudzaŵelengela cuma cake comwe anasiila akapolo ake ku mapeto kwa cisautso cacikulu . Cifukwa cake n’cakuti amatikonda . Mwa thandizo la mzimu wa Mulungu , tingavale mokwanila “ umunthu watsopano , ” umene umaphatikizapo khalidwe la cimwemwe . ( Aef . 4 : 24 ; Agal . Monga mmene taonela , Khrisimasi ni kukondwelela tsiku la kubadwa , ndipo Akhristu oyambilila sanali kucita mwambo wacikunja umenewu . ( Neh . 8 : 1 , 8 , 9 ) Nehemiya sanali kuyang’anila ena mowapondeleza . ( Genesis 1 : 9 , 10 ) Kenako ‘ udzu , zomela zobala mbewu monga mwa mtundu wake ndi mitengo yobala zipatso ’ zinaonekela . Kukamba zoona , Yehova wationetsa kukoma mtima kwake kwakukulu m’njila zosiyana - siyana . Koma kodi n’zothekadi kukonda Mulungu ngakhale kuti sitimuona ? Mogwilizana ndi yankho limene atate wa m’citsanzo cathu anapeleka , Mose anati : “ Inu Yehova , . . . mapili asanabadwe , kapena musanakhazikitse dziko lapansi ndi malo okhalapo anthu , Inu ndinu Mulungu kuyambila kalekale mpaka kalekale . ” Iye adziŵa bwino cibadwa ca anthu ndi maganizo ao . ( Onani polemba kuti MABUKU > MAVIDIYO ) Masiku ano , iye akalephela kupita ku misonkhano ndi mu ulaliki , mwamsanga amayesetsa kuyambanso kucita zimenezo . Baibulo limakamba kuti banja lake linali ndi ziŵeto , koma sanali anthu amalonda oyenda ndi gulu la ngamila . Zinali zoonekelatu kuti pamene tinasintha umoyo wathu , tinapatsa Yehova mwai wotidalitsa . ” Ku nthambi kumeneko , abale amene anasankhidwa ndi Bungwe Lolamulila anali kubwelelamo m’ziyamikilo zimenezo ndi kusankha woyenelela . Ndiphunzitseni kuyenda m’njila zanu . Ndiyendetseni m’coonadi canu ndi kundiphunzitsa , pakuti inu ndinu Mulungu wa cipulumutso canga . Ngakhale n’conco , Paulo anakondwela kuona kuti mnyamatayo anali wodzipeleka . Kuyendela nthambi ya ku Togo pamodzi ndi m’bale Daniel Sydlik ndi mkazi wake Marina , mu 1977 Komabe , anthu ena oona mtima anayesetsa molimba mtima kumasulila Baibo . Patapita nthawi , ndinabwelela ku Madrid cifukwa ndinapeza nchito , kenako ndinakwatiwa . Ndinali kutsutsa zakuti iye aziphunzila Baibulo ndipo ndinali kukoka fodya pamaso pake . N’nali kuona kuti zimene zinacitika zinali zopanda cilungamo cifukwa atate anali munthu wosalakwa . Conco , tingadzifunse kuti , ‘ Ningacite ciani kuti nikhale munthu wauzimu n’colinga cakuti nipeze madalitso monga amene abalewa anafotokoza ? ’ ( Mat . 6 : 33 ) Kuti Akristu akhale okhulupilika afunika kupewa kutengako mbali mu mikangano ndi m’zocitika zina za m’dzikoli . — Yes . 2 : 4 ; ŵelengani Yohane 17 : 11 , 15 , 16 . Koma atapanduka , Baibo imam’chula dzina lomuyenelela kuti Satana , kutanthauza “ Wotsutsa , ” komanso Mdyerekezi , kutanthauza “ Woneneza . ” — Mateyu 4 : 8 - 11 . Baibo siikamba nthawi imene ubwenzi wawo unayamba . A Zimba : Sindinali kudziŵa tanthauzo la lembali . Ndipo pogwilitsila nchito mzimu woyela , Yehova angapeleke mphamvu yofanana kwa mtumiki wake aliyense , mosasamala kanthu za ciyembekezo cimene ali naco . 8 : 46 - 50 ) Yehova pokhala Bwenzi lathu lacikondi , amalimbikitsa anthu oona mtima amene amafuna kum’tumikila koma amalephela kudziletsa pa zinthu zina . Kuti mudziŵe mmene Yehova anathandizila ena a iwo , tiyeni tikambilane za abale na alongo amene akutumikila ku Madagascar , cisumbu cacinayi pa zisumbu zikulu - zikulu pa dziko lapansi . Pamene ndinazidziŵa bwino Mboni za Yehova , ndinazindikila kuti io ali pa ubale wa padziko lonse lapansi . ( 1 Akor . 11 : 1 ) Iye sanali kucititsa manyazi anthu ena kapena kuwakakamiza kucita zinthu zinazake . Mwacitsanzo , malinga ndi Cilamulo ca Mose , Alevi sanali kulandila coloŵa mofanana ndi Aisiraeli ena onse . Malangizo akuti tiyenela kukhala na zolinga zauzimu sakhudza acicepele cabe . ( Onani cithunzi pamwamba . ) ( b ) Ndani amawacititsa ? Tidziŵa bwanji ? Magazini imeneyi amalembela makamaka Mboni za Yehova , koma tilinso ndi magazini ena amene amalembela anthu onse . Motani ? [ Zinenelo 56 ] 4 : 44 . Olo kuti nthambi za m’fanizoli ziimila Akhristu amene adzakhala na moyo kumwamba , fanizoli lili na mfundo zopindulitsa kwa atumiki onse a Mulungu . 89 : 15 , 16 . Zinali zopweteka mtima kwambili . Nayenso Josephus , wolemba mbili waciyuda wa m’zaka 100 zoyambilila , anakamba kuti ciphunzitso cimeneci si ca m’Malemba Oyela , koma “ ni cikhulupililo ca Agiriki , ” cimene anaona kuti n’cozikidwa pa nthano zabodza . Kodi Marthe analimbikitsiwa bwanji pa nthawi imene anali kuvutika maganizo ? Kucita zimenezi n’kutaya nthawi ndi zinthu zopanda phindu . ( Salimo 130 : 3 ) Kupitila m’Mau ake , iye amatipatsa malangizo ambili acikondi na citsogozo kuti atithandize kudziŵa zimene tingacite tikalakwa kapena ngati ena alakwa . Paulo anasiya nchito yake kuti aike maganizo ake pa “ zinthu zofunika kwambili ” Malemba amenewa ndi malemba ena anandithandiza kuti pang’ono ndi pang’ono ndikhale munthu wamtendele . Tica wamkuluyo anavomela , ndipo izi n’zimene zinali kucitika mpaka mkulu wanga anatsiliza sukulu . ( Ekisodo 10 : 12 - 15 ) Dzombe limene Yohane anaona likuimila Akristu odzozedwa amene akhala akulengeza uthenga wamphamvu wotsutsa cipembedzo conama . ( Ŵelengani Aroma 12 : 3 . ) Tingadziŵe mmene Yehova amationela mwa kuganizila zimene Yesu anacita atumwi ake atalakwitsa zinazake . N’ciani cinacititsa cidwi mlongo wina ponena za coonadi ? Mulungu watipatsa mwai wokhala ziwiya ‘ zoumbidwa ndi dothi , ’ zosungilamo zinthu zamtengo wapatali , umene ndi utumiki . ( 2 Akor . Mosiyana ndi anthu amene anafunsa Yesu funso lokhudza msonkho , Jeffery anaphunzila kuthetsa maganizo olakwika pocita zinthu ndi Akristu anzake ndi anthu ena . ( 1 Timoteyo 2 : 9 , 10 ) Malangizo amenewa angathandize atumiki onse a Yehova , kuphatikizapo amuna . Tingacitenji kuti tithandize apainiya apadela ? Yehova amadziŵa bwino mavuto amene atumiki ake akukumana nao , ndipo saiŵala kukhulupilika kwao N’ciani cingatithandize kudziŵa ngati timakonda kwambili Khristu ? ( Maliko 1 : 39 , 40 ) Mwamunayo anali wodwala kwambili moti Luka , amene anali dokotala , ananena kuti munthuyo anali “ wakhate thupi lonse . ” ▪ Kodi ‘ Mumamvetsa Tanthauzo la Malemba ’ ? Mulungu Anamucha Mfumukazi ( Sara ) , Na . Mwacitsanzo , anapilila mayeselo ndi kukhalabe wokhulupilika pano pa dziko lapansi , ndiponso anapeleka nsembe yake ya dipo kwa Yehova mu 33 C.E . Komabe , anafunika kuyembekezela mpaka mu 1914 kuti ayambe kulamulila . ( Mac . 2 : 33 - 35 ; Aheb . Munthu akakhala mkulu si ndiye kuti wakhala wangwilo . ( Num . Abale na alongo athu amenewa ni amene adzatithandiza pa nthawi ya mavuto . ( Aefeso 4 : 24 ) Ndiyeno m’madzulo , n’nabwelela ku hotela kumene n’nali kukhala , ndipo n’napeza cibwenzi canga cakale cikuniyembekeza pakhomo la cipinda canga . Nthawi zambili sin’nali kugona usiku , ndipo n’nali kupemphela uku nikugwetsa misozi , kucondelela Yehova pa mavuto amenewa . Kodi Ayuda anafunika kudziona monga ofunika kwambili cifukwa cakuti anali mbadwa za Abulahamu ? ( Ŵelengani Aheberi 4 : 16 . ) Tinagwilizana kuti aliyense ali ndi cikumbumtima , ndipo tifunika kucigwilitsila nchito posankha zosangulutsa ndi anthu amene tifunika kucita nao . ” — Ŵelengani Aroma 14 : 2 - 4 . Iwo anafuna kuti azikaŵelenga Mau a Mulungu , kuwaphunzila , na kuwakambilana popanda kukakamizidwa zokhulupilila . Katherine anati , “ Ndisanawauze zimene ndinali kuganiza , a Doris anandiuza kuti anali ndi vuto lina limene anafuna kuti tikambilane . Conco , Paulo analimbikitsa ophunzila pogogomezela kuti kukhulupilika kumabweletsa mphoto . Kapenanso mungapatule masiku angapo pa wiki kuti muziyenda kukathandizako nchito pa Beteli kapena pa ofesi ya omasulila mabuku . 20 “ Tiyeni Tilimbikitsane , Ndipo Tiwonjezele Kucita Zimenezi ” A nkhosa zina amadziŵa zimenezi , ndipo amatumikila Yehova pamodzi ndi gulu limeneli . M’bale wina wa zaka 24 amene anabatizidwa ali wacicepele , anati : “ Ndikanatha kuyembekezela kuti ndikuleko mpaka nditamvetsa zinthu mozama . Kenako , tinabwelelanso ku England kukathandiza pa nchito yomanga pa Beteli ya ku London . Nanga anacokela kuti ? Abusa okhulupilika amenewa amatsogoleledwa na mau “ olondola ” opezeka m’buku ya Mulungu . ( 1 Tim . Munalila , koma amayi anu atakutonthozani ndi kukukupatilani mwacikondi , munamvelako bwino . ( Yeremiya 38 : 7 , 8 ) Ndipo Mwiitiyopiya akufotokozedwa kuti anali woyang’anila cuma . Imfa inakhalapo monga cilango cosamvela lamulo la Mulungu . Kunyada kungaticititse kudana ndi uphungu kapena kuukana mmalo movomela modzicepetsa . Mwacitsanzo , mkulu wina amene watumikila paudindo kwa nthawi itali anati : “ Munthu wamanyazi angamangike akakhala na munthu wansangala . ( Gen . 1 : 26 ) Koma pali malile . Kapena mumakhulupilila kuti anthu akhoza kudzilamulila okha ? — Gen . Ndi amene anacititsa kuti zinthu zonse m’cilengedwe zizigwila nchito ndipo ndi amenenso anakhazikitsa malamulo akuti ziziyendela . Iye anasinthadi . Koma kodi n’zinthu ziti zimene tingacite potengela citsanzo cawo ? Tili ndi cidalilo conse kuti iye adzatipatsa zonse zimene anatilonjeza . — Aroma 8 : 32 . Mwacitsanzo , ganizilani za mtsikana wina , dzina lake Kim . Zonse zidzaonongedwela pamodzi ndi dziko la Satanali . Kodi n’cifunilo ca Mulungu kuti ife anthu tizifa ? Tinadabwa ndi kukongoka kwake , kucolowana kwa cipangidwe cake , ndi kuti matupi ake anali athunthu bwino - bwino , ndendende ndi twamoyo tumene tuliko lelo . ” Pofuna kutikonzekeletsa kuimba , cigawo ciliconse pa msonkhano wacigawo kapena wadela cimayamba na mbali ya mamineti 10 ya nyimbo . Kodi Mboni za Yehova Ndani ? Pamene anali ndi miyezi itatu , anayamba kukunyuka mpaka anali kufika pokomoka . Kodi amandiweluza malinga ndi maonekedwe anga , kapena amaona zoposa pamenepa ndipo amandimvetsa bwino kwambili ? ’ [ Cithunzi papeji 4 ] 18 “ Ngati Kingsley Wakwanitsa Inenso Ndingakwanitse ” Koma pali makhalidwe enanso okhumbilika ndi ocititsa cidwi , kuonjezela pa cikhulupililo cimene Rabeka anali naco . Iye analemba zilembo zina za Ciheberi m’mau akuda kwambili . Kodi Mau a Mulungu angacepetse bwanji nkhawa zathu ? ( Ŵelengani Mlaliki 5 : 12 . ) Iwo amafunika kuzindikila kuti Yehova Mulungu ali na mphamvu yoika malamulo alionse amene waona kuti ni acilungamo , oyenelela , ndi osapondeleza . Tiyelekeze kuti a Zulu ndi a Mboni , ndipo afika pa khomo la bambo Zimba . ( 1 Tim . 3 : 1 ) Paulo ‘ sanaleke kupemphelela ’ Akristu a ku Kolose kuti akhale odziŵa zinthu za Mulungu molondola , ‘ kuti aziyenda mogwilizana ndi zimene Yehova amafuna , kuti azimukondweletsa pa ciliconse . ’ ( Akol . Malo ndi Nyumba : Mungapeleke ku gulu la Yehova malo ndi nyumba zoti zingagulitsidwe . Komabe , ubale wanga na Mulungu komanso kukhala m’gulu la abale la padziko lonse , zidzakhala kwamuyaya . Komabe , zinali zovuta kuti lilembedwe m’zinenelo zina cifukwa anthu ambili oŵelenga zinenelozo sanali kulidziŵa liu la Ciheberi limeneli . Motelo , kuti tidzakhale m’dziko latsopano , tifunika kupitilizabe kupilila . Ciukililo cimeneci cidzacitika “ pa nthawi ya kukhalapo ” kwa Khristu . N’cifukwa ciani takamba conco ? Atateyo akumuyankha kuti : “ Palibe amene anapanga Mulungu . Mukadzidziŵa bwino , simungagonje mukakumana ndi ziyeso zimene zili monga cimphepo camphamvu Iwo anali ndi mwai wodzaza dziko lapansi ndi anthu ena angwilo . Kabukuka kapezekanso pa www.jw.org . Iye anaona ubwino wogaŵa Baibulo kukhala m’macaputala ndi mavesi . Mtumwi Yohane anati : “ Mulungu anatisonyeza ife cikondi cake pakuti anatumiza m’dziko Mwana wake wobadwa yekha kuti tipeze moyo kudzela mwa iye . Iye anakamba kuti : “ Mpaka lomba sinikamba bwino - bwino citundu ca Cirasha . ” Koma cifukwa ca kupanda ungwilo kumene tinatengela kwa Adamu , timakonda kucita zinthu modzikonda . 1 Petulo 5 : 5 Mlongo winanso dzina lake Rhonda anakumana ndi mavuto aakulu . Pamene mwamuna wake wosakhulupilila anali kukonza zothetsa banja lao , mlongosi wake anadwala matenda oopsa amene amayamba cifukwa ca kusokonezeka kwa citetezo ca m’thupi . Mofananamo , Mulungu amatisamalila kwambili makamaka pamene tavutika maganizo ndipo tifunika cisamalilo . Mwacitsanzo , pamene Afarisi anaona Yesu akudya cakudya kunyumba kwa Mateyu , anafunsa ophunzila ake kuti : “ N’cifukwa ciani mphunzitsi wanu amadya limodzi ndi okhometsa msonkho ndi anthu ocimwa ? ” 26 : 27 , 28 . ( Mlal . 5 : 10 ) Anthu aconco sakhutila na ndalama zimene amapeza , ndipo pofuna kudziunjikila ndalama zambili , amadzibweletsela “ zopweteka zambili . ” — 1 Tim . 3 : 4 , 5 . Tsopano “ iye ali kudzanja lamanja la Mulungu , pakuti anapita kumwamba , ndipo angelo , maulamulilo , ndi mphamvu zinakhala pansi pake . ” Kukhala paubwenzi wabwino kwambili ndi anthu a mumpingo kungatithandize kugaŵana zinthu ‘ zolimbikitsa . ’ Timacita cidwi podziŵa kuti Yehova , amene ni wamkulu koposa m’cilengedwe conse , ali na khalidwe labwino la kudzicepetsa . ▪ Anthu adzakhala akuononga dziko lapansi pamene Mulungu adzacitapo kanthu . — Salimo 92 : 7 ; Chivumbulutso 11 : 18 . Mosiyana na maluŵa opanga , maluŵa eni - eni amasintha . Pa cifukwa cimeneci , zofalitsa zathu zimalembedwa m’Cingelezi , kenako zimamasulidwa m’zinenelo zina . Yesu anakamba kuti : “ Masiku adzakufikila pamene adani ako adzamanga mpanda wazisonga kukuzungulila . Adaniwo adzakutsekeleza ndi kukusautsa kucokela kumbali zonse . Pamene Solomo anawayesa mwa kulamula kuti mwanayo amudule pakati , mayi wake weni - weni anamvela cifundo . 48 : 18 ) Mwa kuyang’ana zacilengedwe , Nowa anaona umboni wosatsutsika wakuti Mulungu alipo . Anathanso kudziŵa makhalidwe ake osaoneka na maso , monga “ mphamvu zake zosatha ndiponso Umulungu wake . ” 8 : 31 , 32 ; 1 Yoh . 4 : 1 ) Ngati timacikonda kwambili coonadi , zimakhala zosavuta kunyamula “ codzitetezela pacifuwa , ” kutanthauza kutsatila miyezo yolungama ya Mulungu mu umoyo wathu . ( Sal . 111 : 7 , 8 ; 1 Yoh . Lomba , Allen wayamba kuzoloŵela kukhala mu mpingo watsopano umene anakukilako , umene uli pa msenga wa makilomita 1,400 , kucoka kwawo . Onani Nsanja ya Olonda January 15 , 2007 , tsamba 31 . Komabe , “ Mwini zokololazo , ” Yehova , wasonkhezela abale na alongo ambili ocokela m’maiko ena kupita ku Myanmar kukathandiza pa nchito yokolola mwauzimu imeneyi . Dziko la Myanmar lili kum’mwela cakum’maŵa kwa Asia . Monga mmene tidzaonela , yankho ni iyayi . Kwa munthu wotelo , mau a Yehova amveka pang’ono . Yesu ndi citsanzo cabwino kwambili ca munthu amene anaonetsa cikondi codzimana cotelo . Ni yofunika ngako kuposa cinthu ciliconse cokondweletsa cimene anthufe tingapeze . Tulilani Yehova Nkhawa Zanu Zonse , Dec . MUKAONA munthu wateleleka n’kugwa , kodi inu simungasamale poyenda pa njilayo ? Iye anati : “ Ndimakonda Atate . ” Koma samadalitsa zosankha zimene sizigwilizana ndi cifunilo cake . Ndipo samakondwela ngati tasiya utumiki winawake popanda cifukwa comveka . — Ŵelengani Aheberi 11 : 6 ; 1 Yohane 5 : 13 - 15 . Anali kuyembekezela nthawi imene Yehova adzathetsa zoipa zonse ndi kupanga dzikoli kukhala paladaiso . M’malomwake , aika cidalilo cawo pa mabungwe a anthu kuti ndi amene adzathetsa mavuto padziko . 51 : 14 . Ngakhale kuti Jairo amafunika kumucitila zinthu zonse , makolo athu amamukumbutsa kuti moyo wake sudalila pa thandizo la anthu cabe , komanso la Mulungu . Koma anacita zimene zinapulumutsa iye ndi a m’banja lake . — Yos . Akatelo , anthu sangakayikile zimene akucita . A Zimba : Zoonadi , ndifunika kukaŵelenganso nkhaniyi kuti ndiimvetsetse bwino . Pa Yesaya 41 : 8 - 13 , timaŵelenga kuti iye anali bwenzi la kholo loyamba Abulahamu . Paulo anafotokoza kuti : “ Muziyenda modzicepetsa nthawi zonse , mofatsa , moleza mtima , ndiponso mololelana m’cikondi . Muziyesetsa ndi mtima wonse kusunga umodzi wathu mwa mzimuwo , ndi mwamtendele monga comangila cotigwilizanitsa . ” Izi ziyenela kuti zinamuvutitsa maganizo . Mulungu Angakulimbikitseni 6 Kodi tingaonetse bwanji kuti timayamikila mphatso zonse zimene Yehova amatipatsa ? Kumeneku ndiye kucita zinthu mwanzelu . Pa Danieli 12 : 9 pamati : “ Mauwa asungidwa mwacisinsi ndipo atsekedwa ndi kumatidwa kufikila nthawi ya mapeto . ” Kodi Paulo anaonetsa bwanji kuti anali kuyamikila abale ake ? Koma cofunika kwa Akristu ndi ‘ kusiyanitsa pakati pa cinthu copatulika ndi coipitsidwa , ’ kuti akhale ndi khalidwe loyela limene limakondweletsa Mulungu . Kukonda zinthu zakuthupi kungatilepheletse kutumikila Mulungu mwacimwemwe . 37 : 5 , 7 ) Adzadalitsa khama lathu lofuna kulambila iye yekha monga Mbuye woona . Paulo anadziŵa kuti anali pafupi kuphedwa . ( Yes . 40 : 26 ) Popeza kuti Yehova ndi wa dongosolo , iye wakhazikitsa atumiki ake padziko lapansi , ndipo afuna kuti naonso azicita zinthu mwadongosolo . N’nangociphunzila mwa kumvetsela abale akamalalikila na pamisonkhano . M’nkhani ino , mau akuti “ anthu othaŵa kwawo ” amene taseŵenzetsa akutanthauza anthu amene akakamizika kuthaŵa n’kukakhala m’dziko lina kapena m’dela lina m’dziko lawo lomwelo cifukwa ca nkhondo , kuzunzidwa , kapena masoka . Zinali ngati kuti ucimo “ wamyata pakhomo ” kum’dikilila . Pamene mtumwi Paulo anali ku Kaisareya , mmeneli Agabo anam’cenjeza kuti akapita ku Yerusalemu akamangidwa , ngakhale kuphedwa kumene . Conco , Mateyu anaonetsa mzele wobadwila wa Yosefe , umene ndi banja lacifumu la Davide , mmene Yesu woyenelela mwalamulo kukhala pa mpando wacifumu , anali kudzacokela . Apa Yesu anali kutanthauza kuti kulambila koona kwa Akristu sikudalila pa nyumba iliyonse kapena malo ena ake monga Phili la Gerizimu , kacisi wa ku Yerusalemu , kapena malo ena ake opatulika . Inde n’zotheka . Magalamafoni naonso anathandiza ofalitsa ambili kuyamba kulalikila monga mmene makadi a ulaliki anacitila . Tifunika ‘ kudziyesa kuti tione ngati tikali olimba m’cikhulupililo . ’ Vuto lina n’lakuti maboma amenewa amadana ndi Ufumu wa Mulungu , umene unayamba kulamulila mu 1914 . Akristu odzicepetsa amapewa kufuna kukhala ochuka m’dziko lino . 18 : 15 . Ganizilani izi : Ngati nkhosa ziŵili zili pa phili , zina ziŵili zili m’cigwa , ndipo ina imodzi ili kwina kwake , kodi tingati nkhosa zisanu zimenezi ndi gulu ? N’ciani cidzacitika pambuyo pakuonongedwa kwa zipembedzo zonyenga ? Ngakhale zinali conco , iwo anacoka bwino - bwino monga kuti asilikaliwo sanali kuwaona . Anawaphunzitsa kuti afunika kukhala acifundo . Nanga angakonzekele motani misonkhano ? Umu ni mmene Yehova anatilengela . Mulungu pofuna kukumbutsa anthu ake cifukwa cake anawamasula mu ukapolo wa ku Babulo , anatumiza mneneli wake Zekariya mu 520 B.C.E . Mwacionekele , mumalembelana makalata ndi kutumilana foni kaŵilikaŵili . Izi zinandisangalalatsa kwambili . Komabe zinali zovuta kuti ophunzila kapena aphunzitsi achule pamalo enieni m’Mabaibulo ao pamene panali kupezeka mfundo imene anali kufuna . ( 2 Tim . 4 : 2 ) Inde , tiyeni tipitilize kugwila nchito yathu mokangalika , ndipo tizicitila cifundo “ anthu , kaya akhale a mtundu wotani . ” ( 1 Akor . 7 : 28 ) Ngati mwamuna kapena mkazi wanu ni wosakhulupilila , nkhawa na mavuto zimakhala zoculukilapo m’banja . Ngati akamba za Ufumu , ambili a io amangokamba kuti Ufumu uli mumtima mwa munthu . Anaona monga kucita zimenezi kungandicititse kusintha maganizo . Koma Yehova sangam’pusitse . Poyamba , mtumwi Petulo anali na cizoloŵezi cogwilizana ndi Ayuda okha - okha . 15 : 45 . Ukakhala ndi mavuto , m’pamene umafuna anthu pafupi nawe . ” ( Genesis 13 : 14 - 17 ) Kodi tiphunzilapo ciani ? Koma awa anali malo ena , a kufupi na ku Kadesi , kumalile na Dziko Lolonjezedwa . Kungakupatseni mwayi woona makhalidwe ake abwino , amenenso Yehova anaona pamene anamukokela m’coonadi . Kapena ndimayesetsa kukonzanso ubwenzi wathu ? ’ Kodi tifunika kukhala na mtima wotani ? Nkhani iyi idzafotokoza zinthu zofunika zimene zingatithandize kupeza citonthozo panthawi ino ndi mtsogolo . Koma Satana amafuna kuti tiziganiza kuti ndife acabecabe ndipo Mulungu ndi Yesu satikonda . Zimene Tiphunzilapo pa Fanizo la Matalente Yehova anapeleka citsanzo cabwino kwambili pankhani ya cikondi mwa kupeleka dipo . Mwacitsanzo , anthu amatha kukondana , kucitilana cifundo , ndi kukomelana mtima . 5 : 19 - 21 ; 2 Tim . 3 : 13 ) Koma ise pokhala atumiki a Yehova , timafuna - funa nzelu yocokela kumwamba , imene ni yopanda tsankho komanso imalimbikitsa mtendele . Nakhala nikulandila makalata ocokela kwa abale na alongo a ku Ireland , Britain , kuphatikizapo a ku America . Mwacitsanzo , pamene Mboni ya ciyela inapita kudziko lina , inasiya ana ake m’manja mwa banja la anthu akuda . ( Yohane 6 : 44 ) Mwacitsanzo , mmodzi wa anthu amenewo anali Mfarisi wina dzina lake Saulo , amene anali “ wonyoza Mulungu , wozunza anthu ake ndiponso wacipongwe . ” 16 : 3 ; 1 Akor . 9 : 19 - 23 ) Mofanana ndi Timoteyo , kodi ndimwe wokonzeka kudzimana zinthu zina pofuna kuthandiza ena ? Conco , n’kutheka kuti Luka anaphunzila za udokotala ku Sukulu ya Zacipatala mumzinda wa Leodikaya , umene unali pafupi ndi mzinda wa Kolose . Mwamuna wake anamuuza kuti : “ Pemphela kwa Mulungu kuti akuthandize . ” Koma mofanana ndi abale ndi alongo ena , mwina inunso mumalephela kupezeka pamisonkhano nthawi zina . Ndithudi , Yesu angakuthandizeni kupilila nkhawa , ndi kukupatsani ciyembekezo na kukulimbikitsani . — Aheb . 18 : 1 - 4 ) Cifukwa ca kudzicepetsa kwao , Yehova anawathandiza kumvetsa zinthu zozama za m’Baibulo mwa mzimu wake woyela . 40 : 1 ) Mwina ena mwa akapolowo anaphedwa kumeneko m’dela la Benjamini , kumenenso Rakele anaikidwa m’manda . Iwo ali na njila yosungila malangizo owathandiza kugaŵikana na kupanga maselo ena . Komanso angakuthandizeni kudziŵa zimene mungacite kuti imwe na okondedwa anu mukhale na tsogolo labwino . Wamasalimo Davide anali kusinkhasinkha ali pabedi usiku . Yehova nthawi zonse amatiteteza monga gulu kuti mdyelekezi asativulaze . Mkati mwake munali khadi la ku banki , pasipoti , ndi ndalama zambilimbili . M’nthawi ya atumwi , mtumwi Paulo anauza akulu mumpingo wa ku Efeso kuti : “ Mukhale chelu ndi kuyang’anila gulu lonse la nkhosa , limene mzimu woyela wakuikani pakati pao kukhala oyang’anila , kuti muŵete mpingo wa Mulungu , umene anaugula ndi magazi a Mwana wake weniweni . ” ( Mac . Kuonjezela pamenepo , anthu a Yehova akhala akugwilitsila nchito Mabaibulo osiyanasiyana ndiponso kuwagaŵila . Banja lina litafunsidwa kufotokoza cimene cawathandiza kukhala osangalala mu cikwati cao , Sid anati : “ Cikondi ndi khalidwe lalikulu limene takhala tikuyesetsa kukulitsa . Baibo imatiuza kuti : “ Pamene tinali ocimwa , Khristu anatifela . ” Kodi Yobu anali na ciyembekezo canji ? 33 : 24 ) Imfa nayonso adzaimeza . ( Yes . Nthawi zina pangafunike kusintha nthawi yocita Kulambila kwa Pabanja cifukwa ca mapulogalamu ena a kuuzimu . Conco , nanunso Yehova angakulimbikitseni mmene walimbikitsila ine . ” “ Mzimu woyela ukadzafika pa inu , mudzalandila mphamvu . ” — Machitidwe 1 : 8 . N’zosatheka kufotokoza madalitso onse amene timapeza ngati talandila cilango ca Mulungu , ndiponso ngati titengela citsanzo ca Yehova na Yesu polanga ena . N’nali kuona kuti kutenga mwana wa munthu wina n’kosiyana ndi kukhala ni wanga - wanga . ” Adzawathetselatu . Tikutelo cifukwa taona ubwino wotsatila mau olimbikitsa akuti : “ Kuika maganizo pa zinthu za mzimu kumabweletsa moyo ndi mtendele . ” Yesu anafotokoza fanizo la munthu wamalonda amene anali kufuna - funa ngale . Mau Amene Anali Atanthauzo Kwambili ( “ mwanawe ” ) , Nov . Anthu okonda zauzimu amayesetsa ‘ kutsanzila Mulungu . ’ ( Aef . ( Sal . 119 : 142 ) Mwa ici , ufulu wodzisankhila zocita sunapatse mphamvu Adamu ndi Hava zophwanya lamulo la Mulungu . 1 : 3 , 4 ) Yehova angatsitsimule maganizo ndi mtima wathu . Kodi anthu amene adzapilila adzalandila mphoto yotani ? Mosasamala kanthu za mavuto ao , io anali osangalalabe . Popeza ‘ sitingaongolele mapazi athu , ’ tingayambe kutsogoleledwa ndi mau a Yehova kapena mau a Mdani wake . ( Yer . Kodi muona kuti mudzalemela kapena mudzasauka ? Poopa zam’tsogolo , munthu angalephele kapena kucita ulesi kusamalila wacibale amene akudwala . Kodi Satana waonetsa bwanji kuti ndi wonyada kwambili ? Koma acicepele amene amaika patsogolo zolinga zauzimu , akadzakula adzakhala okondwela kuti anapanga zosankha zabwino pamene anali kukula . Mtumwi Paulo anakamba kuti Timoteyo anaphunzila coonadi kuyambila ali wakhanda . Mwacitsanzo , zolemba zina zaciyuda zimafotokoza kuti panthawi ina m’zaka 100 zoyambilila , mtengo wa nkhunda ziŵili zopelekela nsembe unakwela kufika pa dinari imodzi ya golide . Cinthu cimeneco ni nzelu zocokela kwa Mulungu , zimene ngakhale “ golide woyenga bwino sangapelekedwe mosinthana nazo . ” — Yobu 28 : 12 , 15 . Pambuyo pakuti Namani mkulu wa asilikali wacilitsidwa matenda ake akhate , iye anafuna kupatsa mphatso mneneli Elisa , koma mneneliyo anakana . Ndiyeno n’nali kuyembekezela moleza mtima kuti aniyankhe , mwina kwa masiku angapo , olo kwa miyezi . Kodi iye analola kuti anthu a ku Babulo amusinthe ndi kufooketsa cikhulupililo cake ? Imeneyo ibwele kwa iwe ngati ingathe kukupulumutsa pa nthawi ya tsoka . . . ( Gen . 3 : 23 , 24 ) Mwakutelo , Yehova potsatila cilungamo , anacititsa kuti akumane ndi zotulukapo za cosankha cawo . Kodi Yehova adzapitilizabe kutisamalila ? Baibulo imati : “ Pamene ucimo unawonjezeka , kukoma mtima kwakukulu kunasefukilanso . Kodi cilengedwe cimaonetsa bwanji ulemelelo wa Yehova ? Iye anati : “ Ndidzaimbila Yehova moyo wanga wonse . Ndidzaimba nyimbo zotamanda Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga . ” M’malomwake , nimaseŵenzetsa nthawi na mphamvu zanga pokwanilitsa zolinga zauzimu . ” Koma amayamikila kwambili anthu amene amadzipeleka mofunitsitsa cifukwa comukonda ndi mtima wonse ndiponso cifukwa coyamikila kwambili zimene amawacitila . ( Yohane 17 : 15 ) Mwina mumationa tikugwila nchito , tikupita kusukulu , ndi kugula zinthu m’dela limene timakhala . 41 : 3 . Mulungu anakonza zakuti “ mbewu ” ya “ mkaziyo ” ikawononge mngelo woyamba kupanduka ameneyo . Kwa ine , izi zinali monga nthano ndipo n’nati , “ Tiye tiyembekezele mpaka abwele kukatifotokozela zambili . ” 3 : 15 ) Ndiyeno , mudzakhala okhutila podziŵa kuti mwateteza coonadi ca m’Baibulo molimba mtima . M’nthawi ya Mose , mtundu wa Isiraeli unafunikila malangizo atsopano . Tikacita zimenezo tidzadalitsidwa ndi Yehova , ndipo adzatithandiza kucita zinthu mwacikondi . — Aroma 8 : 26 , 27 . Ine ndinabatizidwa m’caka ca 1968 ku Queensland . Ganizilani citsanzo ca Habakuku , amene anauzidwa kuti alosele za kuonongedwa kwa Yerusalemu . Tifunika kukhala oganiza bwino ndi kupewa kukhulupilila zilizonse Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Cikondi n’coleza mtima ndiponso n’cokoma mtima . M’malo mwake , kutumikila Yehova kuyenela kukhala patsogolo pa umoyo wanga . Iye anali “ munthu wofatsa kwambili kuposa anthu onse amene anali padziko lapansi . ” Iye anadziŵa kuti kuseli kwa mapili aja ku Heburoni n’kumene kunali nyumba ya makolo ake . Ndi ciyembekezo cosangalatsa citi cimene tili naco ? Koma pamene mtolo wake unadzuka n’kuima cilili , mitolo ya abale ake inadzuka ndipo inazungulila mtolo wake n’kuyamba kuuŵelamila . ( Aroma 8 : 6 - 8 ) N’zotheka kukhala munthu wauzimu olo kuti ndise anthu opanda ungwilo . ( Aroma 8 : 25 ) Mfundoyi ikhudzanso Akristu onse amene ali ndi ciyembekedzo ca moyo wosatha . ( Aef . 6 : 11 - 13 ) Ndiponso timacita zilizonse zimene tingathe kuti titamande Yehova mwa zocita zathu . 40 : 34 ) Cimeneci cinali cizindikilo cakuti Yehova anasangalala ndi nchitoyo . ( b ) Kodi nkhani ino yatithandiza bwanji kumvetsa fanizo la matalente ? Simufunika kucita kumuona Yesu kuti akuthandizeni . Popeza kuti asilikali aciroma komanso Aciyuda anali atacoka mu mzinda , Akhristu amene anamvela cenjezo la Yesu anatuluka mu Yerusalemu na kuthaŵila ku mapili kupitilila Mtsinje wa Yorodano . — Mateyu 24 : 15 , 16 . Mosiyana ndi Yesu , ife ndife opanda ungwilo ndipo timalakwitsa . Ambili a inu mungakonde kuyambanso kuona bwino kuti muziŵelenga ndi kukhalanso ndi mphamvu kuti muzipezeka pa misonkhano , koma mukuona kuti n’zovuta kapena n’zosatheka . Kodi wabodza angakhalenso ndani , kuposa amene amatsutsa kuti Yesu ndiye Kristu ? ( Yak . 2 : 15 - 17 ) Thandizo limene abale ndi alongowo anapheleka linali la panthawi yake . Cynthia ndi ana ake analimbikitsidwa kwambili cakuti patapita miyezi 6 anacitako upainiya wothandiza . — 2 Akor . Nili na Livija ( b ) N’cifukwa ciani kudzicepetsa n’kofunika kuti munthu athe kukhululukila ena ? ( b ) N’ciani cingatithandize kuona nchito yolalikila ngati mmene Paulo anali kuionela ? Ena amafuna kukhala na ufulu wolankhula komanso wodzisankhila zocita . Tingasinthe motani mmene timaonela zinthu ? Pelekani citsanzo . Tanthauzo la mau akuti “ soul ” linafotokozedwa mu New World Translation of the Holy Scriptures — With References , nkhani zakumapeto . Kodi ndi liti pamene Kristu anamangilila lupanga m’ciuno mwake , ndipo analigwilitsila nchito bwanji atangolimangilila ? Cisautso cacikulu cikadzafika pacimake , maulamulilo a dzikoli adzaonongelatu mabungwe acipembedzo amene ndi aakulu kwambili kuposa ifeyo . ( Chiv . Kodi timapindula bwanji ngati timvela malamulo a Mulungu ? 20 : 18 ) Caka ciliconse , amasinthana ucheyamani pa mamiting’i awo , ndaŵa palibe memba wa Bungwe Lolamulila amene amaonedwa kuti ni wofunika kwambili kuposa anzake . N’nakulila ku malo amene anthu anali okhumudwa cifukwa cakuti Nkhondo Yaikulu imene inacitika m’delali sinacititse kuti dziko likhale labwino . Mwacitsanzo , iye anacilitsa Yobu amene anali kudwala kwambili cakuti anali kufuna cabe kufa . — Yobu 2 : 7 ; 3 : 11 - 13 ; 42 : 10 , 16 . Allen , anazindikila kuti kukuka sikunamutaitse mabwenzi . Komanso ena a ife anayamba kutipatsa nchito zosavuta . ( Mateyu 24 : 14 ) Ife Mboni za Yehova , timadziŵika padziko lonse cifukwa ca nchito yathu yolalikila . Fanizo la Yesu limatikumbutsa khalidwe la Yehova lochulidwa kambili m’Baibulo . Khalidwe limeneli ni “ kukoma mtima kwakukulu . ” Malangizo ena amene angakuthandizeni kuti muzipindula na phunzilo lanu laumwini ali mu Galamukani ! Pofuna kuthandiza munthu womenyedwayo , Msamariya wacifundo anatila mafuta ndi vinyo pazilonda za munthuyo . Izi zionetsa kuti mwacibadwa anthufe timafuna kukhalabe ndi moyo , ngakhale kuti timakumana ndi mavuto ambili . 1 : 13 ) Sembe analekelela khalidwe loipalo , zolengedwa zonse — kumwamba ndi padziko lapansi — zikanakhudzidwa kwambili . 11 , 12 . ( a ) Ndi zinthu zotani zimene zingacititse Akristu kuvutika kukhalabe okhulupilika ku Ufumu wa Mulungu ? Sara anali na zifukwa zambili zokondela malo amenewa . Yoswa ndi Kalebe ndiwo okha amene anabweletsa lipoti labwino pambuyo pozonda Dziko Lolonjezedwa . 3 : 10 , 11 . N’ciani cingatilepheletse kuthandiza anthu amene akuvutika ? Kodi mkwati ndani m’fanizoli ? 2 : 5 ) Naye Yohane analemba kuti : “ Lamulo [ la Mulungu ] ndi lakuti , tikhale ndi cikhulupililo m’dzina la Mwana wake Yesu Khiristu ndiponso tizikondana . ” — 1 Yoh . 3 : 23 . Muzicilikiza Ulamulilo wa Yehova , June Kodi kukhulupilika kwa Yobu poyesedwa kunakweza bwanji ulamulilo wa Yehova ? Iye ali mnyamata , anagonjetsa Goliyati , cimphona cacifilisiti . M’kupita kwa nthawi , mudzafunika kuonetsa kuti ndimwe otsimikiza mtima kucita zinthu mogwilizana ndi zosankha zanu . Cizindikilo cake cinali ca mthunzi umene unabwelela m’mbuyo . Pambuyo pake , mafumu a ku Babulo anatumiza amithenga kwa Hezekiya . Kwa zaka ndithu , tinali kutumikila m’gawo lopanda ofalitsa , koma tsopano tinali na mwayi wotumikila pamodzi ndi abale na alongo ambili - mbili . Kuuka kwa Yesu kumatitsimikizila kuti anthu amene adzakhala padziko lapansi adzaweluzidwa mogwilizana ndi miyezo yacikondi ya Yehova . Kodi tingapewe bwanji kukhala odzikonda ? Abale a ku ofesi ya nthambi ananiuza kuti , “ Tsopano upita kukatumikila monga woyang’anila dela . ” Yesu anali kudziŵa kuti colinga ca Atate wake cinali cakuti alalikile kwa anthu a mitundu yonse , kuphatikizapo mkazi wacisamariyayo . Ndiyeno , tidzakambilana zimene tingacite kuti tikhalebe na cimwemwe ndi mmene tingacikulitsile . Pambuyo poganizilapo mozama , n’naona kuti Mlengi aliko . ” Satana angaticititse kukhala na mzimu woopa anthu , cizunzo , imfa , ndi zinthu zina kuti atifooketse ndi kuticititsa kuleka kutumikila Yehova . — Yes . ( Yoh . 6 : 44 , 65 ) Conco , kukhala na cikhulupililo mwa Yesu kumacititsa munthu kukhululukiwa macimo . Ndipo palibe aliyense wothaŵila kwa iye amene adzapezeka wolakwa . ” — SAL . Yehova analenga dziko lapansi kuti mukhale zinthu zamoyo . MAKOLO amakondwela kwambili ana ao akabatizidwa . Fotokozani zitsanzo zoonetsa mmene kukhala na maganizo a Khristu kungatithandizile posankha ( a ) munthu wokwatilana naye . ( b ) anthu oyanjana nawo . Pa cifukwa cimeneci , ena anali kuikidwa kutsogolo kwa nkhondo kuti aphedwe . Davide anali wodwala kwambili cakuti sanathe kulepheletsa ciwembu ca Abisalomu . Koma kodi kucita zimenezi ndiye kulalikila kumene Yesu anali kukamba ? Anthu ena amacita nayo mantha . Komabe , zaka sizingacititse kuti munthu apewe “ zilakolako zaunyamata ” zoipa . Kumbukilani kuti pamene Mose anamwalila , Yehova anaika mtembo wake m’manda amene palibe akudziŵa . N’cifukwa ciani tinganene kuti ‘ Mulungu ndiye mpando wacifumu ’ wa Yesu ? Kodi tikudziŵa bwanji kuti ufumu wake ndi wolungama ? ( b ) N’ciani cingatithandize kukhala oyamikila ? Masiku ano , sinilephelanso kugona usiku cifukwa coopa zamtsogolo kapena imfa ” 15 : 14 ) Mtundu watsopano umenewu wochedwa ndi dzina la Yehova , unapangidwa ndi Ayuda ndiponso anthu akunja okhulupilila . 8 : 12 ; Yer . Funso limenelo linandicitsa kuganiza kwambili ndipo linandithandiza kuti ndipitilize kuyesetsa kukhala mwamtendele ndi ena . ( Luka 22 : 43 ) Makolo , tengelani citsanzo ca Yehova mwa kulimbikitsa ana anu nthawi zonse , na kuwayamikila akacita zabwino . Komabe pamakhala zotsatilapo zosiyanasiyana . Kupempha mafuta kumene anamwali opusa anacita kumatikumbutsa kuti aliyense payekha ayenela kukhalabe maso komanso kukhala wokhulupilika Koma olambila Yehova ayenela kucita zonse zotheka kuti pakati pawo pakhalebe mtendele ndi mgwilizano . Mau amene Mulungu anakamba kwa Yobu amakwana macaputa anayi m’buku la Yobu — caputa 38 mpaka 41 . ( 2 Mbiri 19 : 6 , 7 ) Conco mfumuyo inakumbutsa oweluza kuti ngati alola tsankho ndi umbombo kuwatsogolela pogamula milandu , Mulungu adzawaimba mlandu wa zoipa zilizonse zimene zingacitike . Ndi zabwino komanso zosangalatsa kwambili abale akakhala pamodzi mogwilizana ! ” Kusinkhasinkha za Yehova ndi Yesu kudzakuthandizani kukhalabe wacangu potumikila Mulungu Iwo amamvela Yesu ndipo amaika nchito yolalikila pamalo oyamba mu umoyo wao . Nikulimbikitsa mabanja ena kuti nawonso ayeseko kukatumikila ku gawo losoŵa monga kuno ku Myanmar . ” Makolo ali ndi udindo wolela ana ao “ m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake . ” Lonjezo la cikwati ( Onani palagilafu 14 ) “ Amacititsa Kukhala ” : Yehova ndiye analenga zinthu zonse ndipo angathe kukhala ciliconse cimene afuna kuti akwanilitse colinga cake . Paulo anayelekezela mpingo wacikristu ndi ‘ nyumba yaikulu , ’ ndipo anayelekezela anthu a mumpingo ndi “ ziwiya , ” kapena kuti zinthu za m’nyumba . Olo zinali conco , tinapilila podziŵa kuti ciliconse , ngakhale imfa , sicingalekanitse Daniel na cikondi ca Yehova . Kukamba zoona , ngati tikhulupilila Yehova kwambili tidzayambanso kum’konda kwambili . ANTHU OLOSELA ZAMTSOGOLO amanena kuti ali ndi mphamvu yodziŵa zamtsogolo . Kodi madokotala ambili avomeleza kuti njila yopimilayo kapena mankhwalawo angathandizedi ? Iwo ndi okhulupilika ndipo amapewa mzimu wokonda cuma , ciwelewele , ndi kudzikonda . Ngakhale kuti sizikudziŵika bwinobwino mmene mkanjowo unalili . Zioneka kuti mkanjowo unali wautali , wokongola , wa manja aatali . ‘ ZOVALA ZAKE NDI ZONUNKHILA ’ 3 , 4 . ( a ) Kodi zovala zacikwati zimene Mkwati wavala ndi zotani ? Mark anafotokoza kuti : “ Tinayamba kukhala ndi umoyo wosalila zambili mwa kusiya nyumba yathu ndi nchito yaganyu n’colinga cakuti tiyambe kuthandiza pa nchito zomanga kumaiko ena . ” Mulungu woona amamva mapemphelo . Yambani kucitapo kanthu . Ndi motani mmene tingagwilitsile nchito mafanizo mwaluso mu ulaliki ? ( Mateyu 4 : 8 - 10 ) Kodi tingatengele bwanji Yesu ? Padzakhala anthu abwino otsogolela . ( Sal . Tsiku lina m’baleyo anapatsa foni mkulu wina kuti aigwilitsile nchito , ndipo zithunzi zamalisece zinaonekela pafoniyo . 6 Ni Mphatso Iti Yoposa Zonse ? N’cifukwa ciani tiyenela kuteteza mtima wathu ? Komabe , sizikuoneka kuti ukapolo wa Ayuda kweni - kweni unacitila cithunzi zimene zinali kudzacitika kwa Akhiristu . ( 1 Akorinto 13 : 5 ) Komanso ngati tikhululukila ena , Yehova nayenso adzatikhululukila . Atate wathu wakumwamba ndi wacikondi . Kuŵelenga nkhani ya Yehosafati kuyenela kutilimbikitsa kudzifufuza . ASIA : Mu 1995 , anthu 502 anafa m’sitolo ina yaikulu mumzinda wa Seoul , ku South Korea . Tsopano iye akutumikila monga mkulu . Ndiyeno tidzaone cidzacitike ndi ciani ku maloto ake aja . ’ ” Tiyeni tikambilane cifukwa cake . ( Salimo 42 : 5 , 6 ) Kodi inunso mumamva conco ? Paulo anali wotsimikiza kuti Yehova amakudziŵa kulambila kwa cinyengo . Ndiponso , anali wotsimikiza mtima kuti Yehova amazindikilanso anthu amene amam’mvela . Ndi anthu angati amene anamva Yesu akupeleka lamulo limene lili pa Mateyu 28 : ​ 19 , 20 ? Yehova analenga zinthu zonse 44 : 22 ) Tisaiŵale kuti kupanga cosankha coipa kungavutitse cikumbumtima cathu kwambili , ngakhale pambuyo pakuti tabwelela kwa Yehova . 1 : 1 ) Barizilai anali munthu wacuma . Kenako , onse aŵili anadziikila colinga cokatumikila pa Beteli . 17 : 3 - 5 , 16 ) Kodi n’ciani cidzatsatilapo ? 1 , 2 . ( a ) Fotokozani cifukwa cake zinaoneka kuti Mose anali pangozi . Baibo imafotokoza kuti : “ Ndipo malipilo owombolela moyo wawo ndi amtengo wapatali , moti munthu sangathe kuwapeleka mpaka kalekale . ” ( Luka 21 : 1 - 4 ) Conco , pa nkhani ya kukhala wodziŵika kwa ena , Yesu anali na maganizo osiyana kwambili ndi a anthu ena . A “ nkhosa zina ” amaona kuti ni mwayi waukulu kuthandiza odzozedwa pa utumiki umenewu . ( Yoh . Atate wathu wacikondi wakumwamba adzawaukitsa na kuwapatsa mwayi wophunzila colinga cake , ndi kukhala ndi moyo wamuyaya . ( Mac . 16 , 17 . ( a ) Kodi ciukililo cimatsimikizila bwanji kuti zimene Yesu anaphunzitsa n’zoona ? Misece kapena kuti mijedo ndi limodzi mwa makhalidwe a Satana amene ndi mdani wamkulu wa Yehova . Ndi anthu otani amene tiyenela kugwilizana nao ? ( Yak . 4 : 1 ) Kunena zoona , ngati tilekelela cidani ndiponso mzimu wodziona kukhala wapamwamba kukula m’mitima yathu tikhoza kumalankhula ndi kucita zinthu mosaganizila ena , ndipo tingawakhumudwitse . ( Miy . Mofanana ndi Mose , sitimadziŵa zonse zokhudza malonjezo a Mulungu . “ Dzina lanu liyeletsedwe . ” — MAT . Atatelo anamenya naco madzi a mtsinjewo , ndipo pang’onopang’ono madzi onsewo anagawanika . ” Baibulo Inapulumuka kwa Anthu Ofuna Kusintha Uthenga Wake 6 Ndipo mwa zokamba na zocita zanu , muzionetsa kuti mumatsatiladi mfundo za m’Mau a Mulungu pa umoyo wanu . — Aroma 2 : 21 - 23 . Kodi inu mumacita ciani mukaona zabwino mwa Mkristu mnzanu ? Mosakaikila , Isaki anayamikila Yehova cifukwa copeleka mwana wankhosa kuti apelekedwe nsembe m’malo mwa iye . Mkhiristu aliyense afunika kukhala woona mtima . Kodi Akhristu oyambilila anali na mbili yanji ? Koma anthu oyela a Yehova amadziŵa kuti Mlengi ndiye amadziŵa mmene tiyenela kugwilitsila nchito magazi . ( a ) Kodi masiku ano cikondi cazilala m’njila ziti ? 19 , 20 . ( a ) N’ciani cimene okwatilana angacite kuti banja lao likhale lolimba ndi lacimwemwe ? Tingacite zimenezo mwa kusinkhasinkha Mau a Mulungu , kupemphela nthawi zonse , ndi kutangwanika ndi zinthu zakuuzimu . Ndipo ngati mphepo ikukuntha , anthu anafunika kukhala pa mtunda osacepela mamita 45 kucokela pamene pali munthu wakhate . 11 : 41 ; 16 : 23 ) Otsatila ake oyambilila anapemphela kwa Mulungu osati kwa Yesu . ( Mac . Luis anati : “ Nimapemphela kwa Yehova kaŵili - kaŵili . Nanga colinga ca moyo n’ciani ? ’ ( Agalatiya 5 : 22 , 23 ) Limodzi mwa makhalidwe amenewa ni cikondi . Ndiyeno , anali kuuza kamnyamatako kuti : “ Ufuna ndalama iti apa ? ” Yesetsani kumvetsa mmene mfundo za mu autilainiyo zikugwilizanilana ndi malembawo . Cikwati ni mgwilizano wopatulika . Solomo analemba kuti pali “ nthawi yoseka ” ndi “ nthawi yodumphadumpha mosangalala . ” 3 : 16 - 19 ; 4 : 1 ) Mwacionekele , lonjezo limeneli ni mbali ya colinga ca Mulungu . Khulupililani dipo . 4 : 36 , 37 ) Abale otsogolela mumpingo anali kumulemekeza kwambili Baranaba , ndipo iye anathandiza Paulo . Anali kugwila nchito ziŵili ndipo tsiku lililonse anali kuuka 4 koloko m’maŵa . Nkhani iyi idzafotokoza zinthu 9 zimene tingacite zoonetsa kuti tili na cikondi “ copanda cinyengo . ” — 2 Akor . Pamene Mulungu anafuna kuti anthu amene sanali Ayuda akhale Akhristu , mngelo anaonekela kwa Koneliyo mkulu wa asilikali wa Aroma m’masomphenya , na kumuuza kuti aitanile mtumwi Petulo kunyumba kwake . — Machitidwe 10 : 3 - 5 . Anthu amene amakamba zinenelo zina ayamikilanso kwambili kukhala ndi Baibulo la Dziko Latsopano m’zinenelo zao . Tikupemphani kuti muŵelenge mosamalitsa nkhani yokamba za masomphenya amenewa . Iwo analibe nazo kanthu kuti nsembe zao sizinali kukondweletsa Mulungu . Timayamikila ngako anchito odzipeleka amene ali kaliki - liki pa nchito zomanga ( Onani palagilafu 11 ) Kungakuthandizeninso kukhala na cidziŵitso cozama ca Mau a Mulungu . N’cifukwa ciani gulu la Yehova likukula kwambili masiku ano ? Tsiku lina pambuyo pa Phunzilo la Nsanja ya Mlonda pa Mande , tinalandila mlendo amene sitinayembekezele . ( Salimo 133 : 1 ) Ena mumpingo anakanidwa ndi abale ao akuthupi kuphatikizapo makolo . Abalewo anaika manja ao pa mnyamatayu , kuonetsa kuti wapatsidwa udindo wapadela mu utumiki wa Yehova Mulungu . — 1 Timoteyo 1 : 18 ; 4 : 14 . Mayeselo ena amabwela mwacindunji kuti afooketse cikhulupililo cathu ndipo ena mwakabisila . M’maiko ena , tapitanso ku makhoti pofuna kuteteza ufulu wathu wa kulambila Yehova ndi kulalikila poyela . ( Machitidwe 10 : 34 , 35 ) Ici ndico cilungamo cimene tonse tingayembekezele kwa Mulungu , amene “ amakonda cilungamo ndi ciweluzo . ” — Salimo 33 : 5 . [ Cithunzi papeji 31 ] Zaka zothela za ulamulilo wa Asa zinali za nkhondo zokhazokha . Nsanja ya Mlonda ino , idzakuthandizani kumvetsetsa bwino colinga ca Mulungu cokhudza anthu na dziko lapansi , na zimene muyenela kucita kuti mupindule na colinga cimeneci . Iye anapitiliza kukhala waukhondo ndi wooneka bwino . Mwacitsanzo , ganizilani zimene zinacitikila wacicepele wina wa zaka 12 , dzina lake Milan ndi a m’banja lake kuciyambi kwa zaka za m’ma 1990 . Abale athu ena akuvutika cifukwa ca matenda , ukalamba kapena cifukwa cakuti anavulala . Izi zinawacititsa cidwi moti anayamba kundikomelako mtima . Nanga tidzapeza madalitso anji tikacita zimenezo ? Konrad Mörtter anamuuza kuti aziseŵenzela kucipatala . Reinhold Weber anapatsidwa nchito ya unesi . Kutalitali . Mwacitsanzo , ganizilani liu la Ciheberi lakuti נפשׁ ( limene kachulidwe kake ni ne’phesh ) , kutanthauza “ moyo . ” ( Onani cithunzi pamwamba . ) ( b ) N’cifukwa ciani Petulo analimba mtima panthawiyo ? Zinthu zinafika poipa kwambili nditafika zaka 20 . Pakuti aliyense wocita zimenezi ndi wonyansa kwa Yehova . ” Mwina akaziwo anali kucita zimenezi . . . , koma si zimene Luka ananena . ” Iye wakhala m’coonadi zaka 30 tsopano . Nkhaniyo inakamba kuti bungwe lolamulila la m’nthawi ya atumwi , inapatsa mphamvu oyang’anila oyendela kuika abale paudindo . Enanso amatumikila monga apainiya apadela , amishonale , alangizi a masukulu ophunzitsa atumiki a Mulungu , kapena atumiki a pa Bwalo la Msonkhano kapena pamalo ocitila sukulu yophunzitsa Baibo . Atumiki onsewa anacita Lumbilo la Kumvela ndi Umoyo Wosalila Zambili . Kwa zaka 20 , Irene wakhala akulalikila mwakhama anthu okamba citundu cimeneci . Kodi n’ziti maka - maka zofunika kupewa ? N’ciani cimene mneneliyo anacita ? Yehova amandiŵelengela , ” anatelo DAVIDE WA KU ISIRAELI , ZAKA ZA M’MA 1000 B.C.E . * Anali kutangwanika na nchito imene Yehova anawapatsa , yomanga cingalawa , kusonkhanitsa zakudya zawo ndi za nyama , na kulalikila uthenga wocenjeza anthu . N’ciani cimene Akristu amene sali pa banja ayenela kudziŵa pankhani ya cisumbali ndi kusankha wokwatilana naye ? Yehova amatipatsa malangizo kuti zinthu zitiyendele bwino . Khalani wokhulupilika . Mukacita zimenezi , zimakhala zosavuta kukhululuka kapena kunyalanyaza ngati wina wakamba kapena kucita zinthu mosaganiza bwino . Kuwonjezela apo , zolakwa zikulu - zikulu zingathetsedwe mosavuta . Anthu amenewa anakwanitsa kucita zinthu molimba mtima , osati cifukwa codzidalila , koma cifukwa codalila Yehova . Kuti timvetsetse , tiyeni tikambilane citsanzo ici . “ Ine Yehova ndine Mulungu wanu , amene ndimakuphunzitsani kuti zinthu zikuyendeleni bwino . ” — YESAYA 48 : 17 . 15 , 16 . ( a ) Kodi “ mdani womaliza ” ndani ? Nanga adzaonongedwa liti ? Ndiponso mu Nsanja ya Olonda ya August 15 , 2012 , tsamba 20 mpaka 29 pa nkhani yakuti “ Samalani ndi Misampha ya Mdyelekezi ” ndi yakuti “ Musasunthike Popewa Misampha ya Satana . ” [ Cithunzi papeji 21 ] wozindikila ? 71 : 9 , 18 . Oksana anakamba kuti : “ Utumiki umenewu wamuthandiza kwambili , cakuti anadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa ali ndi zaka 9 . ( b ) Aja amene ali m’pangano la tsopano ali ndi mwai wotani ? ( 1 Tim . 2 : 4 ) Iye adziŵa kuti anthu amapindula ngako ngati aŵelenga Mau ake m’cinenelo cawo . Mwacitsanzo mu 2014 nyuzipepala ya Bulletin of the Atomic Scientists ya bungwe loona pa za sayansi ndi citetezo inacenjeza bungwe la citetezo la United Nation za zinthu zikuluzikulu zimene zikucititsa mantha anthu . Pangakhale zifukwa zambili . N’ciani cimene Akristu amene ali pa banja ayenela kuphunzila m’Nyimbo ya Solomo ? Yehova Amatsogolela Anthu Ake m’Njila ya ku Moyo , Mar . Kuti tionetse kuti timakonda Yehova sizidalila kuculuka kapena kucepa kwa zinthu zimene tili nazo . Gianni , amene tamuchula poyamba paja , anakamba kuti : “ N’nazindikila kuti zina - zake zasintha . Takamba conco cifukwa cakuti kuŵelengeledwa mlandu na Yehova sikudalila pa kubatizika . Kusankha zinthu mwanzelu kudzatithandiza kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova . Kusadziimba mlandu kungakhale “ kovuta kwambili , ” koma “ n’kofunika ngako ku thanzi la munthu , ” la maganizo ndi la thupi . Izi n’zimene linakamba buku lina lakuti , Disability & Rehabilitation . Pophunzila Baibo , iye angadziyankha molongosoka . Iye analimbikitsiwa ngako mwa kuŵelenga Salimo 46 ; Zefaniya 3 : 17 ; na Maliko 10 : 29 , 30 . Kodi Akhiristu amene ni mabwenzi a Mulungu , amenenso Iye waayesa olungama , nawonso angakhale pa ciopsezo cimeneco ? Kaya munthu wina anatilakwiladi kapena ise ndi amene tili na maganizo olakwika pankhaniyo , tifunika kupemphela kwa Yehova , kum’dalila , ndi kukhalabe wokhulupilika kwa iye . 9 , 10 . ( a ) Tumapepala twauthenga tumatilimbikitsa motani kugwilitsila nchito Baibulo ? Akristu a m’nthawi ya atumwi anali kukonda kwambili Yehova ndi kuyamikila kwambili mwai waukulu umene anali nao wom’tumikila . Pa cifukwa cimeneci io anali osangalala kucita “ utumiki wokhazikitsanso mtendele . ” Ambili anali Akatolika . M’kupita kwa nthawi , amayi anayambanso kuphunzila Baibulo ndipo anabatizidwa . Ndiye cifukwa cake , ngati wofalitsa sangakwanitse kucita zambili mu ulaliki cifukwa ca ukalamba kapena thanzi , angapeleke mphindi 15 , m’malo mwa maola athunthu . Kodi vuto la kusabala lingacititse bwanji munthu kukhala na nkhawa ? ( Luka 23 : 43 ) Angatanthauzenso paladaiso wauzimu amene adzafika pacimake m’dziko latsopano . Nkhondo ndi imodzi mwa zinthu zimene zimacititsa ngozi . Anthu otelo angalephele kulandila madalitso osatha . Adani onse a Yehova “ adzazimililika ndi kusanduka utsi . ” — Salimo 37 : 9 , 10 , 20 . Mlongo Wendy akali ku Vanuatu , ndipo akutumikila pa ofesi yomasulila mabuku . Koma onse ali mbali ya yankho la Yesu lokhudza cizindikilo ca kukhalapo kwake . M’mafanizo onse anai , Yesu anafotokoza zinthu zimene zinali kudzasiyanitsa otsatila ake oona m’masiku otsiliza ano . Kanjele ka mpilu kamaimila uthenga wa Ufumu ndiponso mpingo wacikristu umene ulipo cifukwa colalikila uthenga umenewu . Kumbukilani kuti ngakhale Satana , amene poyamba anali mngelo wangwilo , anacimwa cifukwa colola mzimu wa kunyada kumulamulila . Iye anapita kuti akamufotokozele za nchito ya mtendele imene Mboni za Yehova zimacita m’dziko lake . Angacite zimenezi kupitila m’Mau ake , mzimu wake woyela , ndi cakudya cauzimu cimene timalandila kwa kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . — Mat . Panalinso vuto lopeza ndalama zoyendela kuti tisamukile ku dziko lina . Kodi mkulu angacite ciani kuti akhale ndi nthawi yophunzitsa ena ? Kenako , nkhaniyo inati : “ Mkhristu afunika kucita zimenezi mwa kulalikila uthenga wabwino kwa anthu , ndiponso mwa kutsatila miyezo yolungama ya Yehova mu umoyo wake . ” Zinafotokozanso kuti Satana Mdyelekezi ndi amene amacititsa mavuto amenewo . Timalimbitsa cikhulupililo cathu mwa kupemphela , kuphunzila Mau a Mulungu , ndi kupezeka pa misonkhano . Mwacitsanzo , asilikali asanapite kunkhondo , amaphunzitsidwa mwapadela kuti akhale okonzeka kumenya nkhondo . Nanga tidzapitiliza kuwathandiza kuti aone kuti ndi ofunika ndi kuti akali mbali ya mpingo wacikristu ? — 2 Akor . ( 1 Ates . 5 : 1 - 3 ) Pambuyo pake , padzakhala ciukililo ca padziko lapansi . Mzimu woyela wa Mulungu ndiwo umathandiza Mkhiristu kukhala na cikhulupililo . ( Agal . Masiku ano , Akhristu ambili okhulupilika si odzozedwa , ndipo sanaitanidwe kuti akalamulile pamodzi na Khristu kumwamba . Kukumbukila kuti anthu ena nawonso akulimbana na zofooka zawo kudzatithandiza kukhala nawo paubwenzi . Komabe , ena amene anali kutali ndi mabanja ao sanafune kubwelela . Wacicepele wina Alice Hoffmann ndi mlongosi wake , anali kukakonda kwambili kabuku kao . Popeza kuti Nyumba za Ufumu zinali zitatsekedwa , misonkhano ya mpingo inali kucitikila m’nyumba za abale . Kodi tifunika kucita ciani pakakhala kusintha kwa kamvedwe ka mfundo zina za coonadi ? 2 : 11 ) Mzimu wa dziko umasonkhezela anthu kukonda ciwawa na ciwelewele . Cifukwa ca kukoma mtima kwake kwakukulu , iye anatipulumutsa . Wa Yehova . “ Otsatila za mzimu amaika maganizo awo pa zinthu za mzimu . ” — AROMA 8 : 5 . Masiku ano , munthu angacite daunilodi magazini ya Nsanja ya Mlonda pa webusaiti ya jw.org kapena angaiŵelenge pa JW Laibulale , imene ipezeka m’zitundu zambili . Nthawi zonse adzapeleka njila yopulumukila kuti tikwanitse kuwapilila . Kwa zaka zambili , Yehova wakhala akukamba momasuka ndi atumiki ake m’zinenelo zosiyanasiyana . Paulo ndi Sila anali kugwilako tu nchito twina kuti azidzithandiza . Pezani nthawi yabwino ndi malo oyenelela kuti mulangize ana anu , ndipo citani zimenezo mokoma mtima Komabe , “ Yehova anaicititsa khate mfumuyo moti inakhalabe yakhate mpaka tsiku limene inamwalila . ” Mwacitsanzo , ngati tili na nkhawa kwambili cifukwa ca zolakwa zathu , kodi sitilimbikitsiwa tikaŵelenga kuti , “ magazi a Yesu . . . akutiyeletsa ku ucimo wonse ” ? ( 1 Yoh . Kuti wocimwayo aonetse umboni wokwana wakuti walapadi zoona , payenela kupita nthawi yokwanila . Conco , kodi aliyense wa ife akucitapo ciani ? Pamene munthu wina anafunsa Yesu kuti lamulo lalikulu ndi liti , Yesu anakamba kuti : “ ‘ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi maganizo ako onse . ’ Mfumukazi ya ku Sheba itapita kukamuona Solomo , inati : “ Sindinakhulupilile mauwo mpaka pamene ndabwela n’kuona ndi maso anga , ndipo ndaona kuti ndinangouzidwa hafu cabe . Nanga n’ciani cingathandize okalamba kukhalabe acimwemwe ? Ngozi zacilengedwe zimapha anthu ambilimbili kaya akhale olakwa kapena ai . EL SALVADOR Mabanja aŵili akucita ulaliki wapoyela poseŵenzetsa tumashelufu twamawilo . Iwo ali pafupi na imodzi mwa mashopu akulu - akulu ku San Salvador Patapita caka cimodzi , Arthur anabwela , ndipo anaikidwa kukhala woyang’anila cigawo , cimene cinaphatikizapo Scotland , kumpoto kwa England , ndi Northern Ireland . Komabe , ndisanacoke ku United States , anandipempha kugwila nchito ndi woyang’anila dela wina kwa milungu inai . Colingaco ndi kulambila Mulungu ndi kuthandiza ena kuphunzila za iye . Koma popeza kuti anali kuseŵela chesi kumapeto kwa mlungu uliwonse , sanali kupeza nthawi yopita muutumiki ndi kumisonkhano . Kodi mungakonde kuiŵelenga kuti muone mmene ingakuthandizileni ? Davide anali kuganiza kuti Uriya akapita kunyumba kwake ndi kugona ndi mkazi wake , Bati - seba , anthu adzayamba kuona kuti mwana ni wa Uriya . Iye anaona ndodo imene Davide ananyamula , koma sanaikileko nzelu kuti ananyamulanso gulaye . Baibo imati : “ Mnyamatawe [ kapena mtsikanawe ] , sangalala ndi unyamata wako , ndipo mtima wako ukusangalatse masiku a unyamata wako . ” ( Mlal . KINGSLEY atangomugwila paphewa , anayamba kuŵelenga Baibulo . Iyi inali nthawi yake yoyamba kukamba nkhani mu Sukulu ya Ulaliki . Koma ngati amangocita zinthu mwacidule panchito kapena kugwilako pang’ono cabe , sakhala wosangalala . ” Koma zolinga zopelekela moni n’zolingana . Koma zinanivuta ngako kuti nileke kupepa fwaka . Pambuyo pake , m’caka ca 607 B.C.E . , mzinda wa Yerusalemu unaonongedwa ndi Ababulo . Ndipo mafuko aŵili a Aisiraeli , amene anali kupanga ufumu wa kum’mwela wa Ayuda , anagwidwa ukapolo ndi kucoka m’dziko lao . ( Sal . 89 : 14 ; 119 : 128 ) Ngakhale kuti Satana amakamba kuti ulamulilo wa Yehova ni wolephela , iye wakangiwa kukonza zinthu padziko kuti pakhale cilungamo . Anatumiza mmishonale wina , dzina lake Nani , amene anabwela ndi njinga yake yamoto . Yesu anayankha funso limeneli pamene anati : ‘ Mwana wa munthu anabwela . . . kudzapeleka moyo wake dipo kuombola anthu ambili . ’ Ngakhale kuti tsopano ndili ndi zaka 91 , ndikali kuwakumbukila bwino mau amenewa . M’baleyo anayankha mau oipa ndi kuzimitsa foni cifukwa anali wokhumudwa ndi zimene woyang’anila wakale wa dipatimentiyo anam’citila . ▪ Konzekelani Kudzakhala m’Dziko Latsopano Mfundo imeneyi ikudzutsa mafunso aŵili awa : Kodi Yehova ndi Atate wathu motani ? Phale lokhala na mau amenewa linapezeka m’dela la kufupi na ku Asidodi . Atumiki othandiza naonso amathandiza kuti mpingo ukhale wogwilizana . Mpake kuti Asa anauzidwa kuti : “ Mwacita zopusa pankhani imeneyi , cifukwa kuyambila tsopano anthu azicita nanu nkhondo . ” N’ciani cimapangitsa gulu lathu la abale padziko lonse kukhala locititsa cidwi ? Koma oyembekezela Yehova ndi amene adzalandile dziko lapansi . Mwacitsanzo , ganizilani mavuto amene Mfumu Davide anakumana nawo cifukwa cophwanya lamulo la Yehova mwa kucita cigololo na Bati - seba . Nayenso Marian wa zaka 81 wa ku Brazil , anazindikila kuti afunika kusintha zina ndi zina pa umoyo wake . Cifukwa cakuti timakonda Baibulo , timakondanso zofalitsa zathu zimene ndi zozikidwa pa Mau a Mulungu . Cimene cingakuthandizeni kucita izi ni kuganizila zimene inu mukanafuna kuti wina akucitileni mukanakhala kuti ndinu mlendo . 7 : 13 - 15 ) Kuyeletsedwa kwa odzozedwa ndi a nkhosa zina kumacitika nthawi zonse . Ndipo zotsatilapo n’zakuti amapitilizabe kukhala ndi “ khalidwe labwino . ” 10 : 34 . Cinsinsi Namba 2 Kugwilizana Lemba la Salimo 115 : 16 limati : “ Dziko lapansi [ Mulungu ] analipeleka kwa ana a anthu . ” ( Ŵelengani Zekariya 6 : 13 . ) Uzankoni mzanu wodalilika mmene mumvelela . Kodi atumiki ena okhulupilika a Mulungu anakhala bwanji na mtima wodzikuza ? Ŵelengani Machitidwe 8 : 35 , 36 . Gulu la Mulungu limatithandiza kuti tikwanitse kucita zimenezi . Iye ndi mwana wanga woyamba , tinali kukondana kwambili , ndiponso ndinali kucitila naye pamodzi zinthu zambili . ( Salimo 32 : 8 ) Mwina mungazindikile kuti mwana wanu saoneka wokondwela . Kapena amakonda kukamba zinthu zoipa ponena za abale ndi alongo . Komabe , olo kuti makolo amayesetsa kuphunzitsa ana awo , ana ena amam’siya Yehova . 4 : 32 . Iye anaona kuti zimene Gayo anali kucita unali umboni wakuti anali wokhulupilika , cifukwa kuyambila kale - kale atumiki a Mulungu akhala akudziŵika kuti amakonda kuceleza alendo . — Gen . ( Genesis 2 : 15 - 17 ) Koma Adamu ndi Hava anakana malangizo amene Atate wao wacikondi anawapatsa . 6 : 33 ) Kuti tidziŵe ngati timaona zinthu zakuthupi ndi zauzimu moyenela , tifunika kudzifunsa kuti : ‘ Kodi nimakondwela na nchito yanga yakuthupi koma zinthu zauzimu nimaziona monga zosafunika kweni - kweni kapena zotopetsa ? ’ Mau a m’zinenelo zoyambilila za Baibo akuti Sheol ndi Hades amatanthauza manda a anthu onse . Mwacitsanzo , ganizilani zimene Yesu anacita . Komabe , kodi mfundo za m’Baibo zingakuthandizeni kupilila mavuto amene sangathe masiku ano , monga matenda osacilitsika kapena cisoni cimene timakhala naco tikafedwa ? Cifukwa ca Mau Ake , tayandikila kwa Yehova ndipo nayenso watiyandikila . ( Yak . Anzake ataona kapepala kauthenga kakuti Achinyamata - Kodi Moyo Wanu Mudzaugwilitsa Ntchito Bwanji ? , anam’pempha kuti awapatseko . Khalidwe laciŵili limene linathandiza anamwali anzelu kukhala okonzeka ndilo kukhala maso . Nanga dipo n’ciani maka - maka ? Tifunika kuimilila mowongoka na kukwezako m’mwamba buku lathu la nyimbo . Dziŵani kuti Yehova amasangalala ndi mapemphelo anu ngakhale kuti simungacite zambili mu utumiki wake . — Miy . ( 1 Ates . 5 : 14 ) Pamene titumikila pamodzi na abale ndi alongo athu , timakhala na mipata yambili yowalimbikitsa . Moyo umenewu unalengedwa m’njila yodabwitsa kwambili cakuti sitingathe kuumvetsetsa . Nanga bwanji ngati akuona kuti agwilitsidwa mwala ? Conco , pa kukwanilitsidwa kwa Chivumbulutso caputala 11 , abale odzozedwa amene anali kutsogolela pamene Ufumu wa Mulungu unakhazikitsidwa kumwamba mu 1914 , analalikila kwa zaka zitatu ndi hafu atavala “ ziguduli . ” Koma Husai sanatelo . Mofanana ndi Nowa , Akhristu odzipeleka amamvela Mulungu mwa kugwila nchito imene wawapatsa . Mu ulaliki , tinali kukumana na mavuto osiyana - siyana . Masiku ano , Yehova salola atumiki ake kumenya nkhondo yakuthupi . Aliyense “ wa tianati ” ndi wofunika kwambili kwa Mulungu . ( Ezara 3 : 10 - 13 ) Koma posakhalitsa , adani anayamba kuletsa nchito yomangayo . Mpukutu wa Yesaya wa m’Nyanja Yakufa , wakhala zaka 2,000 . Tiyeni tione zitsanzo zitatu zimene zionetsa mmene mungagwilitsile nchito Baibulo kuti muone ngati muli “ m’cikhulupililo . ” Zimenezi zidzakuthandizani kudziona moyenela . MKAZI WAMASIYE WOSAUKA N’zomvetsa cisoni kuti Naboti atakana kugulitsa mundawo , Mfumu Ahabu ndi mkazi wake anam’konzela ziwembu zimene pambuyo pake zinawabweletsela tsoka . Satana alibedi cifundo ngakhale pang’ono . Ndi zinthu zina ziti zimene mungakambilane ? Cikhulupililo cotelo , sicidalila pa msinkhu wathu , mphamvu zathu , kapena mmene zinthu zilili pa umoyo wathu . Komabe , Baibulo limanena kuti , Yehova ndiye ‘ analenga zinthu zonse . ’ Kodi akulu ndi atumiki othandiza amaikidwa bwanji pa udindo ? Anthu anali kumudziŵa kuti ndi munthu wolimbikila nchito , ndiponso mkazi wacimwemwe amene anali kufuna kuthandiza ena kudziŵa zimene anaphunzila ponena za Mulungu . Ali pa ulendo wobwelela kwawo , anangoona nkhalamu balamanthu ! n’kum’phelatu pamenepo . — 1 Maf . Kodi zimene zinacitikila mlongo wina zionetsa bwanji phindu locilikiza ulamulilo wa Yehova ? ( Agal . 6 : 1 ) Mwina mwaphunzila kuyang’anila nchito za mpingo , madipatimenti adela , kapena kumanga Nyumba za Ufumu . ( Yak . 1 : 14 ) Mosadziŵa , anthu ambili amacita zinthu mogwilizana ndi colinga cake . Ubatizo woyamba umene timaŵelenga m’Baibo ni uja umene unacitidwa na Yohane M’batizi . Iye ni wokonzeka kupanga ubwenzi wabwino na ise . Ndalama zimenezi zimathandizanso pakacitika ngozi zacilengedwe . Izi zibweletsa funso lakuti , Ngati ciphunzitso cakuti mzimu sukufa n’cabodza , n’ciani cimacitika kweni - kweni munthu akafa ? Kodi ni zinthu ziti zimene timakonda kucitila pamodzi mogwilizana m’cikwati cathu ? ( 2 Mafumu 19 : 35 ) M’nthawi ya atumwi angelo anapulumutsa Petulo , Paulo , ndi atumwi ena mwa kuwacotsa m’ndende . Lembali limandikumbutsa kuti Kristu Yesu anafa “ cifukwa ca ine . ” Paulo anagogomeza kuti tifunika kupewelatu maganizo monga akuti : ‘ Mulungu amamvetsetsa . Koma ngati mudalila malangizo a Mulungu , m’malo modalila cidziŵitso canu kapena nzelu zanu , mudzakwanitsa kulela bwino ana . Nanga n’ciani cimene tingacite kuti tionetse kuti timawamvela cifundo anthu ? Ponena za dziko lapansi , Baibo imakamba kuti : “ [ Mulungu ] sanalilenge popanda colinga , . . . analiumba kuti anthu akhalemo . ” Bungwe lolamulila ca m’ma 1950 Malinga ndi Cilamulo , mkaziyo anali wodetsedwa , ndipo sanafunikile kukhudza munthu aliyense . KUTHA KWA UFUMU : Cikanakhala cinthu codabwitsa ngati munthu akanalosela ndendende za munthu ndi dzina lake amene akanatsogolela kukagonjetsa ufumu wapadziko lonse , ndi njila yacilendo imene munthuyo akanacitila zimenezo nthawi yaitali zimenezo zisanacitike . 133 : 1 - 3 ; Mat . Makope amenewo anali okwela mtengo , ndipo ndi anthu ocepa amene anali kupezeka nao . Yehova yekha ndiye ali na ufulu wocita ciliconse cimene angafune , koma mmene amauseŵenzetsela amatipatsa citsanzo cabwino ngako . Masiku ano , m’mipingo yathu muli anthu a mitundu yosiyana - siyana ndiponso a kumaiko ena . Kucita zimenezi n’kofunika kwambili maka - maka ngati , mofanana ndi Mose , tili na udindo m’gulu la Mulungu . Koma ngati sitisamala , nchito ingasokoneze kulambila kwathu . Tikudziŵa kuti Mulungu amatikonda kwambili ndipo nafenso timafuna kuonetsa kuti timam’konda kwambili . Iye anati : “ Ngakhale lomba , nthawi zina zimanivuta kulamulila mkwiyo cifukwa makolo anga anali kukalipa - kalipa . ” Pamene n’nali na zaka 19 , Bud Hasty amene anali kugwilizana kwambili na banja lathu , ananipempha kuti niyambe kucita naye upainiya kum’mwela kwa America . Kuti umphawi uthe , pafunika boma lamphamvu la padziko lonse limene lingagaŵe cuma ca dziko mosakondela . Tiphunzilapo mfundo zisanu izi : N’zoona kuti kucita zimenezi kumakondweletsa . Kenako Yesu anati : “ Anthu amenewa adzalandila ciweluzo camphamvu . ” M’malo mwake , zimalimbikitsa anthu kudalila dziko loipali la Satana . Nthawi zambili anali kukangiwa kudziletsa . Kuwonjezela apo , angatengelepo mwayi pa zophophonya za atsogoleliwo kuti afooketse asilikaliwo . Ziŵelengelo zionetsa kuti , kuyambila mu 1914 anthu opitilila 100 miliyoni aphedwa pa nkhondo . Ciŵelengelo cimeneci cimaposa ziŵelengelo za anthu onse m’maiko ambili . Koma , nsembe ya Yesu imapeleka moyo kwa onse omukhulupilila . Anthu a m’zipembedzo zambili amakhulupilila kuti mzimu wa munthu sukufa Ndine wofunitsitsa kuuzako ena amene amadziona kuti sangasinthe , za makhalidwe a Yehova amenewa , popeza kuti inenso ndi mmene ndinalili . 10 : 11 . Naboti anakana cifukwa comvela lamulo limene Yehova anapeleka kwa Aisiraeli , lakuti safunika kugulitsilatu colowa ca fuko lawo . ( Lev . 25 : 23 ; Num . ( Yakobo 1 : 4 ) Kodi kupilila kungamalize bwanji “ nchito ” yake mwa ife ? N’cimodzimodzinso ndi anthu ambili a m’maiko amene Baibulo ndi lofala kwambili . Koma pamene munthu amene ndimagwila naye nchito anandifunsa , ndinafuna kuti ndimve zambili . N’zimene Delphine anacita . Mai wina amene ali pabanja , ndipo ali ndi ana , anakamba kuti kuŵelenga Baibulo kunali kumuvuta kwambili . Tsopano pali mitundu iŵili ya ma IUD . ( Yohane 13 : 34 , 35 ) Mtumwi Yohane alembanso kuti : “ Ana a Mulungu ndiponso ana a Mdyerekezi amaonekela bwino ndi mfundo iyi : Aliyense amene sacita zolungama sanacokele kwa Mulungu , cimodzimodzinso amene sakonda m’bale wake . Ndi kusintha kuti kwaposacedwapa kumene kumakusangalatsani kwambili ? Ndinaphunzila mmene ndingakhalile m’komboni imeneyo popeza umoyo unali wovuta . Lemba la Miyambo 3 : 32 limati : “ Munthu wocita zaciphamaso Yehova amanyansidwa naye . ” Iye amanyansidwa ndi munthu amene amazionetsela kuti ndi wokhulupilika , koma amene mwamseli amacita zosalungama . ( Gen . 30 : 1 , 2 ) Amishonale amene amatumikila ku mayiko kumene anthu amakhala na ana oculuka , nthawi zambili amafunsidwa cifukwa cake sakhala ndi ana . MASAMBA 3 - 6 NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO N’ciani cofunika kwambili pa kulambila kwathu ? Kodi kukhala pa mzela wa makolo a Mesiya kunadalila kukhala oyamba kubadwa ? N’cifukwa ciani cilimbikitso n’cofunika ? Kuti io asamuke , anapempha mlongo wina wa mumpingo kuti azikhala m’nyumba yao . Anapemphanso acibale ao kuti azisamalila atate a Kenneth amene ndi okalamba . Ndipo tili ndi zifukwa zomveka zotsatilila malangizo a Yehova paumoyo wathu wonse . Conco , sanapitilize kuphunzila Baibulo . Conco , polalikila ku kunyumba ndi nyumba , tifunikila kulemekeza nyumba za anthu . — Mac . ( Miy . 15 : 22 ) Anthu okonda zinthu zauzimu amenewa angakuuzeni kuti ngati mucita utumiki wa nthawi zonse , mudzaphunzila zinthu zimene zidzakuthandizani pa umoyo wanu wonse . Tiyenela kukhala okonzeka kupatsa anthu moni na kuwalimbikitsa . ( Maliko 10 : 17 , 18 ) Izi n’zosiyana kwambili ndi zimene Herode Agiripa Woyamba anacita . Iye anali mlangizi wa Sukulu ya Giliyadi Yophunzitsa Baibo , ndipo pambuyo pake anatumikila mu Bungwe Lolamulila . Davide anatenga ndodo , cola , ndi gulaye . Anthu amenewo anaukitsidwa ndi matupi aumunthu , ndiyeno pambuyo pake anafanso . 4 : 9 , 10 . Iye amathandizilanso tumagulu twa cinenelo ca Cingelezi , Cichainizi ndi Ciwiga . Dziko la Côte d’Ivoire ( limene kale linali kuchedwa Ivory Coast ) ndiye kumene amalima kwambili nyemba za koko , zimene amapangila cokoleti . Kodi kuphunzila Baibo kungakuthandizeni bwanji inu na banja lanu kukulitsa khalidwe la kudziletsa ? Yakobo 4 : 8 Mukhoza kutumikila Yehova mokwanila mukali acinyamata . Sisera atamva kuti Aisiraeli akufuna kumenyana naye , anacitapo kanthu mofulumila . Kodi kutumikila Yehova ndi “ mtima wathunthu ” kumatanthauza ciani ? Masiku ano , cinyengo cili paliponse kaya m’zandale , m’zacipembedzo kapena m’zamalonda . Ndipo ena amakhumudwa akulu akawapatsa uphungu . Conco , Mkristu akamaphunzila Baibulo , mzimu woyela wa Mulungu umam’thandiza kukhala ndi cidziŵitso cakuya , cikondi cacikulu , ndiponso kulimbitsa ubwenzi wake ndi Yehova . Baibulo imati : “ Ana aamuna a Eli anali anthu opanda pake . Iwo anali kunyalanyaza Yehova . ” Kukhululuka kumaonetsanso kuti munthu ni womvetsetsa . N’nali kulaka - laka kukhalanso na manja , koma n’nali kuona kuti zimene anakambazo ndi maloto cabe ndipo sizingatheke . Iye anakamba nkhani ziŵili zogwila mtima pamsonkhano , komanso anakamba nkhani zisanu zolimbikitsa pa wailesi . Yoswa , mtsogoleli wa Ayuda , ananena za zinthu zimene anthuwo anali kudziŵa bwino kuti : “ Inu mukudziŵa bwino ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse , kuti pa mau onse abwino amene Yehova Mulungu wanu ananena kwa inu , palibe ngakhale amodzi omwe sanakwanilitsidwe . 2 : 19 . 22 : 39 ) Mulungu ndi Kristu afuna kuti tizikonda anzathu . Cikwati cathu n’colimba cifukwa timagwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo . ” Kodi tiphunzilapo ciani pa citsanzo cawo ? Mwina akufunika thandizo lanu kuti alimbitse cikhulupililo cake . Koma cocitika cimeneci sicinali yankho lokwanila la pemphelo lathu lakuti “ Ufumu wanu ubwele . ” ( Mat . Mtumwi Petulo anali mkulu wodziŵika ngako mumpingo wacikhristu . Muziyamikila ngati ena akupatsani uphungu Panthawi imeneyi , tidzafunika kukhala m’malo acitetezo amene Yehova adzapeleka kwa atumiki ake . Panthawi yake yoikika , Yehova adzaloŵelelapo pa zocitika za padziko lapansi , ndipo zimenezi zidzacititsa kuti anthu ake aukilidwe . Mmodzi mwa asayansi amene analimbikitsa ciphunzitso cimeneci ni Lord Kelvin . Mmodzi wa anzakewo anali Husai , amene Baibo limati anali “ mnzake wa Davide . ” Ndani [ wa milungu yao ] pakati pao amene anganene zimenezi ? Colinga ca nkhani ino ndi kukambilana mfundo zimenezi kuti tidziŵe mmene tiyenela kuonela Nyumba za Ufumu , mmene tingacilikizile nchito yomanga nyumba zimenezi mwa kupeleka ndalama , ndi mmene tingazisamalile . ZAKA zingapo zapita , mwamuna wina ndi mkazi wake kudziko la Fiji anali ndi nchito yapadela yoitanila anthu ku Cikumbutso ca imfa ya Kristu . Ganizilani za Yoswa . Komabe , pewani kukulitsa nkhani zing’ono - zing’ono , cabe cifukwa cakuti simunakondwele na zimene mwana wacita . Ndithudi , Satana ndi “ mkango wobangula . ” Ndipo mofanana ndi moto , zimene timakamba zingabweletse mavuto aakulu . Baibulo lili ndi miyezo ya Mulungu imene ili monga pulani , ndipo tingatsatile miyezo imeneyi paumoyo wathu . ( 1 Akorinto 14 : 26 ) Ndipo tikamakambilana nao misonkhano isanayambe kapena itatha , timalimbikitsidwa cifukwa timadziŵa kuti tili ndi mabwenzi ambili amene amatikonda . — 1 Akorinto 16 : 17 , 18 . Yehova anayang’ana m’busa wodzicepetsa ameneyo , amene anali kugwila nchito ya pansi yoboola nkhuyu , cakudya cimene cinali kuonedwa kukhala ca anthu osauka . Tikamalankhula momasuka ndi Yehova , tidzatonthozedwa pa mavuto athu . Ndiye cifukwa cake Paulo anapitiliza ndi mau akuti : “ Mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu . ” ( Afil . Kodi timalalikila mmene tingakwanitsile monga ofalitsa Ufumu acangu ? Malinga ngati dziko la Satana lilipo , sitingakwanitse kucitanji ? Koma n’cifukwa ciani zimenezi siziyenela kutibweza m’mbuyo ? ( Yes . 54 : 5 ; 62 : 4 ) Cimeneci ciyenela kuti cinali ‘ cikwati ’ covuta ngako . Sitiyenela kutumikila Yehova uku tikutumikilanso milungu ina kapena kukhulupilila zinthu zina zabodza . Wosimba Ndi Demetrius Psarras Ngakhale n’conco , Yehova mwacifundo cake , angatithandize kukhala mtundu wa munthu amene iye afuna . Mufunika kuganizila mosamala zimene mufuna kukamba , ndi kupeza nthawi yabwino yokamba nao . Koma magaziniyo inagwilitsila nchito mavesi ena a m’Baibulo pofotokoza kuti “ abale ” a m’fanizoli amaimila anthu okhawo amene adzalamulila ndi Yesu , ndipo onse adzakhala kumwamba panthawi ya Ulamulilo wa Zaka 1000 . Nimacigwila na manja aŵili olo kuti nilibe manja . N’cifukwa ciani kukhala woona mtima kumafuna kupewa cinyengo ciliconse ? Mkulu wina dzina lake Ludovic , amene anapindula ali wacicepele pamene ena anamuonetsa cidwi anati : “ Ndimaona kuti ndikamaonetsa cidwi mwa m’bale zimam’thandiza kupita patsogolo mwamsanga . ” Izi zingaonetse kuti munthuyo akupita patsogolo mwauzimu . Kavinidwe kawo komanso zocita zawo pa maphwando , zimakhala zosayenela kwa Akhristu . Komabe , Yesu sanaike maganizo ake pa kusiyana kumene kunalipo pakati pao . M’malomwake , anauza maiyo kuti : “ Mai , ndithu nthawi idzafika pamene anthu inu simudzalambila Atate m’phili ili kapena ku Yerusalemu . ” Ndiyeno mupatseni cipatso ciliconse , mwina apozi , na kum’funsa kuti : “ Kodi udziŵa kuti apozi inapangidwa motsatila ‘ lesipi ’ ? ” Tisaiŵale kuti Mulungu ndiye ‘ adzaika maganizo m’mitima yao kuti cilomboco ciukile zipembezo zonyenga . Ndipo zimenezi zidzacitika modzidzimutsa ndiponso panthawi iliyonse . Kukamba mokhadzula kapena kumulanga msanga - msanga kungacititse manyazi mwanayo cakuti angaleke kumasukila makolo ake . “ Mzimuwo umacitila umboni limodzi ndi mzimu wathu kuti ndife ana a Mulungu . ” — AROMA 8 : 16 . Amangolalikila ena ndi kuwacenjeza za zinthu zimene zidzacitika mtsogolo . Iye sapeleka malangizo oipa . Atadziŵa kuti anthu ambili sanamvepo coonadi ca m’Baibulo , Yeong Sug analabadila mau Yesu a pa Mateyu 24 : 14 akuti : “ Uthenga wabwino uwu wa Ufumu udzalalikilidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse kenako mapeto adzafika . ” Nchito imeneyi ikadzacitika kufika pa mlingo umene Mulungu afuna , ulosi udzakwanilitsidwa wakuti : “ Kenako mapeto adzafika . ” Kaŵili konse , nkhosa za atate ŵake zinafuna kugwidwa na zilombo zolusa . Kuti moni wathu ukhale wolimbikitsa , olo kuti ni wacidule , tifunika kuupeleka mocokela pansi pamtima ndi mwacikondi . Patapita masiku anai , abale ena anamuuza kumene ndinali . 10 : 27 ; Yos . 17 : 15 , 18 ) Anthu ena akamaona malo aakulu amene alibe mitengo masiku ano , amakaikila ngati kunalidi nkhalango . Mwacitsanzo , kwa zaka 300 , Yehova anali kusankha oweluza ndi kuwapatsa mphamvu kuti apulumutse mtundu wa Isiraeli kwa anthu amene anali kuwazunza . 11 : 3 ; Aef . Mwacitsanzo , mlongo wina amene ndi mpainiya wacangu anati : “ Nthawi zambili ndikaganizila mobwelezabweleza zophophonya zanga , ndimadzimva wacabecabe . Pamsonkhanowo , m’bale wa m’Bungwe Lolamulila analengeza za kutulutsidwa kwa Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso m’Cingelezi . Anapitiliza kutumikila Mulungu ngakhale pamene anayang’anizana ndi adani oopsa . Pofika ca kumapeto kwa nthawi ya atumwi , uthengawu unali kupezeka m’mipukutu yosiyanasiyana 66 . Ndipo zosankha zikulu - zikulu zimafunika kuziganizila mosamala ndi kuzipemphelela . Satana amasangalala akaona anthu ochuka akunyoza mphatso ya ukwati yocokela kwa Mulungu . N’ciani cina cingakuthandizeni kuwaphunzitsa kukonda Yehova ndi kum’tumikila ? Pogaŵa nthawi yolambila , makolo ayenela kuganizila zosoŵa za mwana aliyense , maka - maka ngati ali ndi zaka zosiyana . Kucokela panthawiyo , cakhala colinga cathu ‘ kulabadila mocokela pansi pa mtima ’ ziphunzitso ndi miyezo ya Mulungu . WOYANG’ANILA DELA wina anali pafupi kutsiliza msonkhano wake ndi bungwe la akulu . Koma kodi tidzawalezela mtima mpaka atalimbanso ? Ndipo mavuto amangokhala ngati sadzatha moti zimakhala zovuta kupilila . Ngakhale n’conco , anapatula nthawi yokulitsa cidwi ca anthu amene anali kumvetsela uthenga wabwino . Conde lembani penapake zimenezi kuti musakaphonye cocitika cimeneci . Mpaka pano , sindidziŵa ngati mbeu za coonadi zimene ndinabyala zinakula . — 1 Akor . Kodi ena masiku ano amacita ciani mosazengeleza kuti aziteteze mwa kuuzimu ? * Mwina , koma sitingakambe motsimikiza . Cifukwa iye ni Mlengi wa zinthu zonse komanso ni Mfumu Yamphamvuzonse m’cilengedwe conse . ( 1 Tim . ( Ŵelengani Afilipi 4 : 13 . ) 11 : 24 - 26 ) Pa cifukwa cimeneci , Yehova anam’dalitsa , ndipo mosakayikila m’tsogolo adzalandila madalitso ena owonjezeleka . Nchito ya maola ocepa imeneyi imamuthandiza kusamalila mkazi wake . 18 Yehova Amatsogolela Anthu Ake ( Mlaliki 1 : 4 ) Komabe , cisautso cimene cikubwela ndi nkhondo ya Mulungu “ yoononga amene akuononga dziko lapansi . ” Pambuyo pakuti takhala angwilo ndi kupyola pa ciyeso cotsiliza , Yehova adzasaina satifiketi imeneyo , titelo kukamba kwake , na kutitenga kukhala ana ake okondeka a padziko lapansi . Mofanana ndi manyuzipepala , wailesi inatithandiza kufikila anthu ambili m’malo amene munali ofalitsa ocepa . 4 : 18 ) Koma zitanthauza kuti tisamaonetse cikondi m’mau cabe , maka - maka ngati munthu wina afunikila thandizo . Anthu ena anali kudziŵa za ciŵembu cimene Davide anakonza kuti Uriya aphedwe . 116 : 3 ) N’ciani cingatithandize kukhalabe ndi mtima woyamikila ? Mosakayikila , nawonso adzapindula na citsanzo canu cabwino . Ayuda anali kusunga mipukutu ya Malemba m’masunagoge awo . Patapita zaka zambili , anthu ena , kuphatikizapo Akhiristu , anayamba kugwilitsila nchito mipukutu imeneyo . — Machitidwe 15 : 21 . Ngati palibe amene atsegula citseko , kodi tingayambe kuyang’ana pa windo kapena kuyamba kuzungulila nyumba kuti tione ngati pali munthu ? Kuyambila pamene ndinali ndi zaka zitatu , madzulo alionse ndinali kupemphela nao limodzi pemphelo limene ena amalicha Pemphelo la Ambuye . Monga tidzaonela m’nkhani yotsatila , mafumu onse anayi amenewa analakwitsapo zinthu zina . M’nkhaniyo , M’bale Sanderson anakambanso za ciyembekezo ca moyo wakumwamba cimene M’bale Pierce anali naco . 26 : 27 ) Baibulo limaletsa kumwa moŵa mopitilila malile ndi kuledzela . ( 1 Akor . Zinthu zabwino za m’cilengedwe zimene timaona , kumva , ndi kudya , zimatipatsa umboni wakuti afuna tizisangalala . 1 : 1 - 3 ) Ngati ndinu kholo lacikhristu , mosakayikila muyembekezela mwacidwi nthawi pamene mwana wanu adzabatizika . — Yelekezelani na 3 Yohane 4 . Ena anakwatilana ndi mtumiki wa Yehova , koma mwamuna kapena mkazi wao anasiya coonadi . Ofalitsa atsopano akhoza kuwonjezela luso lawo lophunzitsa ngati timalalikila nawo . Buku lina linakamba kuti mau akuti “ anasemphana maganizo ” ndi akuti “ anakangana , ” amagwilitsidwanso nchito pofotokoza “ kukangana kumene kumakhala m’khoti , ” ndipo zimenezi zikusonyeza kuti “ Mikayeli ‘ sanalole Mdyelekezi ’ kutenga mtembo wa Mose . ” Enanso amalandila ziphuphu kwa anthu amene amafuna kupeleka ndalama zocepa za msonkho kapena ndalama zina zimene amafunika kulipila ku boma . Awa ni mau amene nthawi zina Yesu anali kuseŵenzetsa pokamba na azimayi . Anthu amene amadya zizindikilo za pa Cikumbutso amadziŵa kuti ali m’pangano la Ufumu . Ngati zinali conco , Dema anataya mwai wamtengo wapatali wa kuuzimu , cifukwa cakuti dziko silikanamupatsa zinthu zabwino kuposa madalitso amene Yehova akanamupatsa cifukwa cokhala mnzake wa Paulo . — Miy . 7 : 9 , 10 ) Yehova adzacitanso cimodzimodzi kwa inu . Lemba la Aheberi 11 : 7 imakambapo za cikhulupililo ca Nowa , amene “ atacenjezedwa ndi Mulungu za zinthu zimene zinali zisanaoneke , anasonyeza kuopa Mulungu ndipo anamanga cingalawa kuti banja lake lipulumukilemo . ” Iye anauza ophunzila ake okhulupilika kuti adzapita kukawakonzela malo kuti akalamulile ndi iye mu ulemelelo wake . 5 , 6 . ( a ) Kodi kunyadila n’kulakwa ? Makhalidwe anu oyela ndi nchito zanu zosonyeza kudzipeleka kwanu kwa Mulungu , ziyenela kuonetsa kuti mumakhulupilila kuti mwapeza coonadi komanso mukufuna kutsatila mfundo za Mulungu . Nanga ndani amene amafuna kuti tifooke ndi kuleka kutumikila Yehova ? “ Ana anga okondedwa , tisamakondane ndi mau okha kapena ndi pakamwa pokha , koma tizisonyezana cikondi ceni - ceni m’zocita zathu . ” — 1 YOH . 3 : 18 . Kukhala na cikhulupililo mwa Yesu amene ni njila ya Mulungu yotipulumutsila , kumasonkhezela wokhulupilila kuuzako ena uthenga wabwino . Popeza kuti sindinakambilane vutoli ndi mkazi wanga , nayenso anali ndi nkhawa kwambili . Ndine wokondwela ngako kudziŵa dzina lake . ( Gen . 2 : 21 , 22 ) Ndiyeno Mulungu anapatsa banja limeneli mwai wodzaza dziko lapansi ndi ana ao . Conco , ataphwanya lamulo la Mulungu iye anayembekezela kuti adzaweluzidwa dzuŵa lisanaloŵe . Lomba , iwo ali na colinga cocita upainiya . Mwacitsanzo , Satana anapaya ziŵeto za munthu wokhulupilika , Yobu , ndiponso atumiki ake . Henschel anabwela kudzacititsa msonkhano ku Malawi kwa nthawi yoyamba , ndipo kucoka nthawiyo cikhumbo cakuti nditumikile Yehova mu utumiki wanthawi zonse cinakula kwambili . Yehova ndi wokoma mtima kwambili . Khalani ndi cidalilo conse kuti Yehova ‘ adzakukhuthulilani madalitso osoŵa powalandilila . ’ — Mal . Onani 1 Akorinto 10 : 13 ; Aheberi 4 : 16 . Citsanzo cao cingatilimbikitse kupilila ngati tili ndi udindo waukulu . Mogwilizana ndi zimene buku lina linakamba , mauthenga osoceletsa “ amagwila bwino nchito yake ngati anthu . . . sakwanitsa kuganiza bwino . ” 6 Maulosi Amene Anakwanilitsidwa Kumeneku sikudziŵa mwacisawawa . Tinalinso kuyesetsa kuthandiza ena pa misonkhano yathu . NYIMBO : 3 , 47 Gail anati : “ Lonjezo limeneli ndi lolimbikitsa kwambili . Ndiponso , zimene gulu la Mulungu la kumwamba limacita zimakhudzanso gulu lake la padziko lapansi . Tsiku lina pamene Jairo anali ndi zaka 16 , Atate anamufunsa kuti : “ Jairo , kodi ufuna kubatizika ? ” Baibulo limati : “ Inu akazi , muzigonjela amuna anu kuti ngati ali osamvela mau akopeke , osati ndi mau , koma ndi khalidwe lanu . ” Tsiku limenelo Akani ndi banja lake anaponyedwa miyala ndipo anafa . ( Yos . Mwacitsanzo , pa miyezi yocepa cabe , mliliwo unapha asilikali ambili a ku America amene anali ku France kuposa amene anaphedwa ndi adani pankhondo . Molingana ndi Msamaliya wacifundo wa m’fanizo la Yesu , timafuna kuthandiza anthu ovutika , kuphatikizapo amene si Mboni . Koma lomba umoyo wanga ni wamtendele , wacimwemwe , ndi wokhutila . ” ( Aroma 12 : 2 ) Mwina timamvela aneba , anzathu a kunchito , ndi a kusukulu , akukamba mau onyoza anthu a mtundu wina kapena a fuko lina . Kodi Yehova anamva bwanji na zimene zinacitika ku Meriba ? N’cifukwa ciani Aroma caputa 8 ni yofunika ngako kwa Akhiristu odzozedwa ? ( Deut . 17 : 18 - 20 ) Tifunika kusinkhasinkha maka - maka zimene Yesu anali kuphunzitsa ndi kuganizila citsanzo cake cabwino ca kutumikila Mulungu modzicepetsa . ( Mat . Ndiyeno afunseni kuti : “ Kuti nonse mukakhale mwamtendele pa cisumbupo , kodi mungasankhe anthu a makhalidwe anji ? ” Iye sanali kufunsa mafunso amene ana onse amafunsa . Koma kodi cinali coyenela iwo kucita zimenezi ? 91 : 11 ) Tikamaganizila madalitso amenewa ocokela kwa Mulungu , cimwemwe cathu cidzakula . — Afil . “ Tikufuna kucita zinthu zonse moona mtima . ” “ Cipulumutso Canu Cikuyandikila ” ▪ Zaka 100 za Ulamulilo wa Ufumu wa Mulungu ( Ŵelengani Mateyu 2 : 13 - 18 . ) Sin’namvetsetse cifukwa cake anacoka panyumba cifukwa tinali kuwakonda kwambili . Kuyambila m’caka ca utumiki ca 2015 , masukulu aŵili amenewa anaphatikizidwa m’kupanga sukulu imodzi , imene imachedwa Sukulu ya Alengezi a Ufumu . Cilimbikitso cimeneco cinapangitsa kuti asadziphe . ( a ) Kodi tifunika kucita ciani kuti tipite patsogolo mwauzimu ? Ndipo kwa nthawi yoyamba mu umoyo wanga , n’nayamba kupezeka pa misonkhano ikulu - ikulu yophunzitsa Baibo . ( Luka 12 : 15 ) Conco , ngati zigaŵenga zamfuti sizinasinthe maganizo awo , ngakhale pambuyo pokamba nazo mofatsa , Akhristu anzelu amatsatila mfundo imene Yesu anakamba , yakuti : “ Usalimbane ndi munthu woipa . ” Monga Yehova * anakukhululukilani ndi mtima wonse , inunso teloni . ” — Akolose 3 : 13 . Ndipo mukaona dokowe , muzikumbukila kuti mufunika kukhalabe chelu kuti mudziŵe tanthauzo la zocitika za padziko masiku ano . Zinali ngati kuti iye wacilitsa mtima wanga . PACIKUTO : Mkulu akuphunzitsa mtumiki wothandiza kucita ulaliki wapoyela wa m’mizinda ikuluikulu m’mbali mwa mseu wochedwa Haiphong Road , mumzinda wa Kowloon Mu Baibulo muli nkhani zambili zimene zionetsa kuti Yehova amaona zabwino mwa atumiki ake . Ndipo nkhanizi zimaonetsanso kuti iye amatha kuona ngakhale maluso ao apadela . Kodi mukudziŵa mmene anaphunzilila coonadi ? Cifukwa ciani ? Kodi n’ciani cingakuthandizeni kuona ubatizo mmene Yehova amauonela ? 3 : 2 , 3 ) Koma zimenezi siziyenela kulepheletsa Mkhiristu kukhala wofatsa . Muzitsatila malangizo ocokela ku ofesi ya nthambi ndi kwa akulu - akulu a boma , kuti musaike moyo wanu kapena wa ena paciopsezo . Mosiyana ndi alangizi a anthu , iye salema na kumvetsela mapemphelo athu , ngakhale titamupempha mobweleza - bweleza kuti atithandize . Taonani , kucokela tsiku limene makolo athu anamwalila , zinthu zonse zikupitililabe cimodzimodzi ngati mmene zakhalila kuyambila pa ciyambi ca cilengedwe . ’ ” — 2 Petulo 3 : 3 , 4 . Mwacitsanzo , dikishonale ina inati “ kukhala wodzicepetsa kumatanthauza kuziona kuti ndife acabecabe pa maso pa Mulungu . ” Masiku ano , Yehova amaticenjeza kupitila m’Nkhani za m’Baibo , zofalitsa , komanso kupyolela m’malangizo ocokela kwa Akhristu anzathu . Ni utumiki wapadela uti umene Paulo anapatsidwa ? Iye amalalikila uthenga wabwino mwakhama ndipo amacita zonse zimene angathe kuti mpingo ukhale wogwilizana . Ndiye cifukwa cake Paulo anati : “ Ndikucita zinthu zonse cifukwa ca uthenga wabwino , kuti ndiugaŵilenso kwa ena . ” ( 1 Akor . Zinatelo kuti tisakhale ndi cikhulupililo mwa ife tokha , koma mwa Mulungu amene amaukitsa akufa . Mukaŵelenga cocitika cina cake mu Buku Lapacaka , imani pang’ono ndi kuganizila zimene mwaŵelenga kuti zikukhudzeni mtima . 12 : 17 ) Colinga cake ndi kumeza anthu a Yehova . 9 : 22 . Tingatsanzile bwanji makhalidwe a Mulungu , monga cikondi ? Kodi acinyamata angacite ciani tsopano kuti adzasangalale ndi mipata yambili yotumikila Yehova mtsogolo ? Mau a Mulungu amanena mosapita m’mbali kuti : “ Musamangidwe m’goli ndi osakhulupilila , cifukwa ndinu osiyana . Pemphani Yehova kuti akucilikizeni muli ndi cikhulupililo kuti adzakuthandizani , ndipo muuzeni nkhaŵa zanu . Cifukwa ca cikhulupililo , iye anacoka mumzinda wa Uri , ndipo anakana kukhazikika mumzinda uliwonse wa ku Kanani . Mau acidule akuti B.C.E . amatanthauza “ Yesu asanabwele , ” ndipo mau akuti C.E . amatanthauza “ Yesu atabwela . ” Koma atakalamba sanali kumva kukoma kwa cakudya ndi mau a nyimbo . ( 2 Sam . ( Miy . 21 : 5 ; Mlal . 9 : 10 ) M’Malemba Acigiriki Acikhiristu , timauzidwa kuti : “ Ngati tingathe , tiyeni ticitile onse zabwino . ” Pocita phunzilo la Baibulo la banja mlungu uliwonse , iye amandiyang’ana ndi kuyang’ana kompyuta yake . Ngakhale pamene ndinali wocotsedwa , ndinali kudziŵa kuti Mboni za Yehova zimaphunzitsa coonadi . ” Ngati wina asankha kukhalabe mbeta , ni nkhani ya mwiniwake atatsimikiza mu mtima mwake . Ndipo amene wasankha kuloŵa m’banja nayenso n’cosankha cake . Gulu lina analicha kuti ndi nkhosa , ndipo gulu lina analicha kuti ndi mbuzi . Dziko lathuli linapulumuka koma “ anthu osaopa Mulungu , ” adani ake , ndi amene anaphedwa . Kumapeto kwa buku la Danieli , timaŵelenga mau olimbikitsa amene Mulungu anamuuza , akuti : “ Iwe pita ku mapeto ndipo udzapuma . ” Kodi timacita bwanji tikapatsidwa uphungu ? Lemba lathu la caka ca 2015 : “ Yamikani Yehova , cifukwa iye ndi wabwino . ” — Salimo 106 : 1 Baibulo limati : “ Patapita nthawi , mfumu ina yomwe sinam’dziŵe Yosefe inayamba kulamulila mu Iguputo . Kodi anthu amene amalandila cilango ca Mulungu ndi amene amacikana ali na tsogolo lotani ? Kodi Yesu anali kucita ciani ndi mikangano ya anthu a m’nthawi yake ? PAMENE Yesu anali kudya cakudya cothela camadzulo na atumwi ake , anali kudela nkhawa kwambili za mgwilizano wawo . Tikuphunzilapo kuti iye ndi Atate ake amaganizila anthu ena . Cimene cingatithandize kucita zimenezi ni kumvetsela nyimbo za mau zopezeka pa webusaiti yathu ya jw.org . Kodi fanizo la matalente limatilimbikitsa bwanji ? ( Yakobo 1 : 17 ) Kodi muganiza kuti Mulungu angatipatse mphatso yabwino kwambili koma yosakhalitsa ? Ngakhale kuti kusintha - sintha nkhani zokambitsilana kumacititsa kulambila kwa pabanja kukhala kosangalatsa , onse ayenela kukonzekela kuti kulambilako kukhaledi kogwila mtima . Baibulo limatiuza kuti Mulungu anapatsa anthu mtima wofuna kukhala ndi moyo mpaka kalekale . Anamuvula zovala pamaso pa apolisi acinyamata . 12 : 5 - 7 ) Kodi Farao akanacita ciani ? Koma abale ndi alongo amene atumikila kwa zaka zambili ali ndi mwai waukulu cifukwa adzionela okha mmene gulu lasinthila . Kucotsa munthu kumateteza mpingo woyela wacikristu . Ndipo tizitamanda Yehova tikaona mmene akudalitsila “ gulu lonse la abale [ athu ] m’dzikoli . ” — 1 Pet . N’cifukwa ciani Yesu anagwilitsila nchito fanizo limeneli ? Atafika m’mudzi mwathu , anagwila anyamata atatu a Mboni . Iwo ataukitsidwa , anakhalanso ndi moyo padziko lapansi . N’cifukwa ciani Davide anali wokonzeka kuyembekezela moleza mtima ? Ndipo cimaniŵaŵa ngako . Amakamba kuti , ‘ Sudzakula , ndiwe cibeketebenzi , cidumbo iwe . ’ ( Mateyu 24 : 45 ) Masiku ano , mabuku ofotokoza Baibulo akupezeka m’zinenelo zoposa 700 . Yehova anali ndi Yosefe , ndipo ciliconse cimene iye anali kucita Yehova anali kucidalitsa . ” ( Gen . Kukhala okhulupilika kwa Yehova ndi Ufumu wake kumaposa mmene timakondela cinthu cina ciliconse . Koma panatenga nthawi komanso n’napeleka mapemphelo ambili kuti nifike popanga cosankha cimeneci . ” Kukambilana zinthu ngati zimenezi kudzathandiza wophunzila kuti asamangoganizila za nchito yake koma aziganizila kwambili mmene anthu ena angapindulile ndi nchitoyo . Kulimbana ndi zofooka zimenezi kuli ngati kumenya nkhondo Paulo anakamba za “ maziko olimba a Mulungu ” pamene anagwila mau a Mose onena za nkhani ya Kora ndi anthu ake ya pa Numeri 16 : 5 . Kodi tingakambilane bwanji ndi Mulungu ? Cotelo , Mkhiristu aliyense ayenela kudzifunsa kuti , ‘ Kodi zimene chechi yanga imaphunzitsa zigwilizana ndi zimene Baibulo imakamba ? ’ Lemba la Aheberi 11 : 13 , imakamba za anthu ena akale kuti : “ Onsewa anafa ali ndi cikhulupililo , ngakhale kuti sanaone kukwanilitsidwa kwa malonjezowo . Koma anawaona ali patali ndi kuwalandila . ” “ Mwana wathu akalakwitsa zina zake , tinali kumutsimikizila kuti timakondwela ndi zabwino zimene anacita m’mbuyomo . Baibulo limaonetsa kuti cikondi cocokela pansi pamtima n’cofunika kuti anthu azisangalala . YEHOVA ni Mulungu wooloŵa manja . Ena atumikila ku maiko acilendo kwa zaka zambili . Conco , uyenela kukumba mozama , ngati kuti ufuna - funa miyala ya mtengo wapatali . Wacicepele ali pafupi kutsiliza sukulu . N’ciani cinawathandiza kukhalabe okhulupilika kwa Yehova ndi kupitiliza kukhala acimwemwe ? Koma kodi n’ciani cinacititsa msonkhanowu kukhala wapadela , ngakhale kuti opezekapo anali 150 cabe ? Conco , io sagwila nchito imene Yesu anayambitsa . Kusamalila banja lanu pa zinthu zakuthupi n’kofunika . Koma cofunika ngako ndi kusamalila banja lanu pa zinthu zauzimu . Aliyense ali na ufulu wothamangitsa motoka mmene angafunile , kapena kuyendela kumbali iliyonse ya msewu . Kodi mungacite mantha ? N’nali na nkhawa cifukwa n’naona kuti ubwenzi wathu tsopano udzatha . Panthawi yachuti , ndinali kuthandiza nchito yokolola , ndipo nthawi zina ndinali kuyendetsa matalakita athu . Kodi simuvomeleza kuti Mdyelekezi “ wacititsa khungu maganizo a anthu osakhulupilila ” kuti asadziŵe kuti mapeto a dzikoli ali pafupi , ndi kuti Khiristu tsopano akulamulila mu Ufumu wa Mulungu ? ( 2 Akor . Tsiku lina mayiyo anaganiza zina zimene zinamuthandiza kuti acile . Kambili , pa maceza aconco m’pamene ena amakhala omasuka kutifunsa zokhudza umoyo wathu . Nanga ni zitsanzo ziti zimene zionetsa kuti Akhristu oona amadalila Mulungu na mtima wonse m’nthawi yovuta ino ? ’ Ndipo tisataye mwayi woseŵenzetsa ufulu umene tili nawo potumikila Yehova mmene tingathele . Ndiponso tiyenela kupewa kuuseŵenzetsa molakwika . Koma timafunika kucita khama kuti tipitilizebe kusintha umunthu wathu . Ndipo “ ansembe ambilimbili anakhala okhulupilila . ” ( Mac . NJILA YOTHETSELA VUTOLI : Ufumu wa Mulungu ukuthetsa ziphuphu mwa kuphunzitsa anthu mmene angacotsele maganizo oipa amene amayambitsa ziphuphu . 102 : 10 . Conco , tiyenela kusonyeza kuti timayamikila cikondi cimene Yehova wationetsa mwa kumukonda na kumvela malamulo ake . — 1 Yoh . 4 : 19 ; 5 : 3 . Enanso amakamba kuti azilanga ana awo mwamphamvu na colinga cofuna kuwathandiza . 6 : 16 ) Kwa zaka zambili , ciŵelengelo ca khamu lalikulu cakhala cikupita patsogolo cifukwa ca dalitso la Yehova . N’cifukwa ciani Mose anali ndi cikhulupililo cakuti adzalandila mphoto ? Ndipo kwa zaka zambili , n’nali pa cisumbali na cigaŵenga cinacake . ” Yehova angatithandize kusintha ndi kuyamba kumutumikila m’njila imene amavomeleza . ( a ) Ndani amene Yehova wapatsa udindo wolela ana ? Isiraeli wauzimu anapindula kwambili ndi malangizo amene Yehova anapeleka kudzela mwa Yesu . Yelekezani kuti muli m’dziko lopanda nkhondo , matenda , kapena imfa . Tikhoza kunolela - nolela luso limene Mulungu anatipatsa ndi kupitiliza kucita nchito zabwino . Baibulo limati : “ Tsutsani Mdyelekezi ndipo adzakuthawani . ” 14 : 31 . Muzipeza nthawi yokamba nao , kudya nao , ndi yoseŵela nao . PA 26 MARCH , 1937 , amuna aŵili olema kwambili a paulendo , anali kuyendetsa thilaki lakuda ndi fumbi pang’ono - pang’ono kuloŵa mumzinda wa Sydney , ku Australia . Ndinazindikila kuti moyo wanga , wa mkazi wanga ndi wa ana anga unali wofunika kuposa zinthu zina . ( Onani kamutu kakuti “ Kodi Anthu Anai Okwela pa Mahachi Alidi pa Liwilo ? ” ) Iye anatumiza Mwana wake wokondedwa kuti abadwe monga munthu wangwilo wofanana ndi Adamu . Tiyeni tione njila ina ya mmene tingatengele citsanzo ca Yesu . ( Aroma 14 : 12 ) Tifunika kucita khama kuti ‘ tisasiye cikondi cimene tinali naco poyamba . ’ Iye anali kuona kuti walephela nchito yake monga mneneli ndi kuti anali wosafunika kwa Yehova ndi kwa anthu onse . Ndani Anagaŵa Baibulo kuti Likhale ndi Macaputala ndi Mavesi ? 99 : 6 , 7 ) Masiku ano , otsalila odzozedwa asanapite kumwamba kukatumikila monga ansembe pamodzi ndi Yesu , amatumikila mokhulupilika m’bwalo la padziko lapansi la kacisi wauzimu . Mwacikondi , Yehova anatikonzela Msonkhano wa Umoyo na Utumiki Wathu n’colinga cakuti tikhale aluso kwambili mu ulaliki . Ndiye cifukwa cake Mau a Mulungu amati : “ Imvi ndizo cisoti cacifumu ca ulemelelo zikapezeka m’njila yacilungamo . ” — Miy . Yehova amatitsimikizila kuti adzatithandiza pa nthawi imene takumana ndi mavuto . Panthawi imodzi - modziyo , woyang’anila nthambi anacita chimo ndipo anam’cotsa paudindo n’kuikapo wina . ( Aroma 8 : 15 - 17 ) Akristu amene ali ndi ciyembekezo cokhala padziko lapansi kosatha amachula Yehova kuti “ Atate . ” Mulungu amatidalitsa ngati tidzicepetsa na kusintha khalidwe lathu ( Onani palagilafu 8 - 10 ) Kodi Yehova anathandiza bwanji Aisiraeli ndi kuwateteza pamene anali kumenyana ndi Aameleki ? Iwo analidi mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu . Phunzitsani ana anu coonadi ca m’Baibo pa mpata uliwonse umene wapezeka ( Onani palagilafu 10 ) Ngati timaonadi kuti kuimba nyimbo ni mbali ya kulambila , tidzapewa kuyenda - yenda kapena kuphonya mbali imeneyi ya misonkhano . Mungadabwe ndipo mungafune kudziŵa cifukwa cake munthuyo akufunsa zimenezo . Lembali limati : “ Khulupililani Mulungu , khulupililaninso ine . ” Mulungu ali na cifukwa cabwino cokhalila wokwiya cifukwa ca citonzo cimeneco . Komabe , Baibo imachula Yehova kuti ni “ wosakwiya msanga . ” N’cifukwa ciani anthu amavutika ndi kufa ? Yehosafati atabwelela ku Yerusalemu , Yehu mwana wa Haneni , wamasomphenya anamudzudzula cifukwa cogwilizana ndi Ahabu pankhondoyo . Cacitatu , Paulo anakamba kuti Ayuda anali “ odzipeleka potumikila Mulungu . ” Kodi mungadziikile colinga cakuti muzilalikila kaŵili - kaŵili ? Komabe , iye walonjeza kuti adzathetsa zoipa zonse , monga mmene nkhani yotsatila idzafotokozela . [ Mau apansi ] Munthu aliyense amasangalala akavala zovala zabwino , makamaka ngati ayenda mu ulaliki , ku misonkhano ya mpingo , kapena ya cigawo . Koma Rubeni anapempha abale akewo kuti asamuphe Yosefe m’malo mwake amuponyele m’citsime copanda madzi ali wa moyo ndi colinga cakuti iye amupulumutse nthawi ina . — Genesis 37 : 19 - 22 . Conco , Cilamulo cinali “ mthunzi cabe wa zinthu zabwino zimene zikubwela osati zinthu zenizenizo . ” ( Aheb . ( b ) Ni madalitso a Ufumu ati amene Yesaya na wamasalimo anakambilatu kuti Mulungu adzabweletsa ? MKULU wina anauza mnyamata wa zaka 12 , dzina lake Christopher kuti : “ Ndinakudziŵa kucokela pamene unabadwa , ndipo ndine wosangalala kumva kuti ufuna kubatizidwa . ” ( Onani pikica namba 2 kuciyambi . ) ( b ) Kodi mkazi amene anali mkati mwa ciwiya aimila ciani ? Pambuyo poti m’bale Russell Poggensee wamvetsa bwino mfundo imeneyi , ndipo wazipenda mosamalitsa , iye anavomeleza kuti : “ Yehova kupyolela mwa mzimu wake woyela sanandipatse ciyembekezo ca moyo wakumwamba . ” Ngati mufuna thandizo kuti mukhale pafupi na Mulungu kapena kuti mupeze citonthozo , pemphani a Mboni za Yehova m’dela lanu kapena lembelani kalata ku ofesi ya nthambi ya kufupi na kwanu . 27 Khalidwe Labwino KwambilI Kuposa Dayamondi Mwacitsanzo , ngati mwana wanu saseŵenzetsa bwino foni , mungamulande foniyo kapena kumuletsa kucita zinthu zina pafoni kwa kanthawi . 5 : 19 - 21 ) Ndipo Yehova analamula kuti onse m’gulu lake afunika kukhala oyela kuthupi na kuuzimu . — 2 Akor . Mu 1931 , atumiki a Yehova anayamba kudziŵika ndi dzina la m’Malemba lakuti Mboni za Yehova , ndipo zimenezi zinawapangitsa kucita zambili pa nchito ya Ufumu . ( Yes . Pa cifukwa ici , oongoka mtima amatha ‘ kumvetsetsa zinthu zolondola , zolungama , zowongoka , ndiponso njila yonse ya zinthu zabwino . ’ Ena amafunsila kwa olosela zam’tsogolo kapena kwa owombeza , amene amati amalosela zimene zidzacitika kutsogolo poseŵenzetsa makhadi a njuga , manamba , kapena mizela ya padzanja . Cinsanja ca mulungu ameneyu cinali kuonekela patali mumzindawu . Anagaŵilanso tumapepala tokwanila 150,000 . Ciitano cimeneco cinalembedwanso m’manyuzipepala , ndi pa matikiti a sitima okwanila 400,000 . Baibo imakamba kuti “ kumwamba ndi kwa Yehova Mulungu . . . , kumwambamwamba ndi zonse zili kumeneko , dziko lapansi ndi zonse zili mmenemo ndi zake zonsezo . ” ( Deut . Komanso timalola Yehova kukamba nafe mwa kuŵelenga Mau ake ndi kuwasinkhasinkha nthawi zonse . Lemba limeneli lifotokoza mmene Akhiristu amadziŵila kuti ni odzozedwa . Limati mzimu woyela umacitila umboni pamodzi na mzimu wawo . Kusintha kumeneku kumasonyeza kuti Yehova ndiye akutsogolela gulu lathu . Tsiku lina , m’ndendemo munacitika congo pamene anthu aŵili ogwila nchito kwa mfumu Farao anawabweletsa m’ndendemo . ( Aroma 8 : 32 Buku Lopatulika ) Yehova anatipatsa amene amakonda kwambili . Pamene anali wacinyamata , anayamba kumwa moŵa mwaucidakwa , ndipo zotulukapo zake anakhala munthu waciwawa . Kuyambila nthawiyi , zinthu zinasintha kwambili ku Ireland . Tiyenela kukonda adani athu mosasamala kanthu za zimene amaticitila Woyang’anila kagulu kanu ka ulaliki katsopano ayenela kuyesetsa kuyendako namwe mu ulaliki mukangofika . Ndiponso , ngati tili ndi cikondi , sitidzakhala wodzitama kapena wodzikuza . Anthu ambili amakonda kunyadila mtundu wao , cikhalidwe , mzinda , kapena dziko lao . Mmodzi wa alendowo anali Mary Zazula , wa ku Edmonton , ku Alberta . Dziko loipali linaŵeluzidwa kale , ndipo ciwonongeko cake cayandikila kwambili . Mu November 1948 , tinacoka mumzinda wa New York kupita ku Bahamas . Tinakwela boti yaitali mamita 18 yochedwa Sibia . Ponena za utumiki wake pa Beteli , Debra anati : “ Nthawi zina ndimadzimva ngati kuti ndili pa zithunzi zopezeka m’mabuku athu zoonetsa anthu akumanga nyumba m’Paladaiso . ” Ndinaganiza kuti akucita maseŵela a pa kompyuta , koma ndinadabwa kum’peza akuŵelenga Baibulo . Eliezere sanachulidwe dzina lake m’nkhani yonseyi , koma aoneka kuti ndiye mtumiki amene anatumidwa . Musamaone Cabe Maonekedwe , June Mwacitsanzo , ngati tinakumanapo ndi mavuto tili ana , kapena ngati pali pano tikukumana ndi mavuto amene amatisoŵetsa mtendele , tiyenela kupitiliza kupilila ndi kucilimika . 7 : 26 - 29 ) Akazi acilendo aciwelewele amene anali kulambila Bala anali kukhala pakati pa Aisiraeli . Ndife okondwela kuti nchito yolalikila za Ufumu yapita patsogolo kwambili . Koma pamene anakana kuloŵa usilikali , anaweluzidwa kuti akhale m’ndende kwa caka cimodzi na hafu , ndipo anakhala m’ndende zokwana 9 zosiyana - siyana . M’malo momuletsa , kambani naye mokoma mtima ndi molimbikitsa . Kodi vesi ili mulidziŵa ? Kodi ndimasonkhana mokhazikika ? 38 : 15 , 16 ) * Kodi tiyenela kucita mantha ? Masiku ano , anthu a Yehova amakondwela kukhala m’paladaiso wauzimu , mmene muli mtendele woculuka . Mofananamo , muzionetsetsa kuti io amapezeka pamisonkhano yampingo , misonkhano ikuluikulu , ndi pa kulambila kwa pabanja . M’malo mowapitikitsa anthu odwala khate , nthawi zina anali kuwagwila ngakhale kuwacilitsa kumene . — Mateyu 8 : 3 . Kuti tipindule ndi macenjezo a Mulungu , coyamba tiyenela kuzindikila kuti amasamala kwambili za ife . ( Chivumbulutso 1 : 8 ) Conco , popeza Mulungu ndi wamuyaya sizitidabwitsa kuti iye ndi Wamphamvuyonse . Mulungu anati : “ Ine ndine Yehova , amene ndimasonyeza kukoma mtima kosatha , ndimapeleka ziweluzo ndi kucita cilungamo padziko lapansi . Abulahamu anayembekezela moleza mtima cifukwa anali na cikhulupililo mwa Yehova . Kodi mumayesetsa kuganizila nkhani yaikulu , m’malo mongoganizila za mavuto anu ? NYIMBO : 101 , 84 Yankho la funso limeneli likukhudza nchito imene iye amakonda kwambili . Kusankhana mitundu kunali kofala pa nthawiyo . ( Mlaliki 7 : 9 ) Tonse ndife ocimwa ndipo timalakwitsa . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Salinso aŵili , koma thupi limodzi . ” — Mateyu 19 : 6 . Conco , kwa iwo kukwatilana ndi wacibululu sikunabweletse vuto lililonse kwa ana amene anali kubeleka . ( Ŵelengani Luka 24 : 21 . ) Mosataya nthawi , abale ndi alongo a ku Japan anayamba kugwilitsila nchito buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu limene linalembedwa mosavuta kuŵelenga . Komabe , kaya timakumana ndi mavuto otani , n’zolimbikitsa kudziŵa kuti atumiki akale okhulupilika a Yehova anali omasuka kufunsa funso limeneli , limenenso ise tingakhale nalo , ndipo Mulungu sanawaimbe mlandu . ( 1 Petulo 3 : 18 ) Ganizilani izi : Tonse tinalandila ucimo kucokela kwa Adamu , ndipo cilango ca ucimo ndi imfa . Mwacimwemwe mtsikanayo anati : “ Cakudya ca ziŵeto tili naco cambili , komanso malo ogona alipo . ” Kumeneko kunali kuceleza kumene iye anaonetsa mwamunayo ndi ena amene anali naye . Mu October 2009 , ofesi ya nthambi ya ku United States inatumiza makalata ku mipingo yonse m’dzikolo . ( Yeremiya 10 : 23 ) Yehova amadziŵa zinthu zotiyenelela . “ Tsopano Yehova Mulungu anatenga munthu uja n’kumuika m’munda wa Edeni kuti aziulima ndi kuusamalila . Tingakonzekele kudzakhala ndi moyo m’dziko latsopano mwa kugonjela makonzedwe a Yehova masiku ano . Koma tifunikanso kuyesetsa kukhala okhutila ndiponso ogwilizanika . Ndiyeno , amaimilila patsogolo pa kacisi wolambilila ndi kutsatila miyambo yao yomwe ndi kuŵelama , kuomba m’manja , ndi kupemphela kwa mulungu wao wamkazi . Ganizilani za nkhondo . Iye anati : “ Nthawi zonse ine sindisintha . ” ( Yesaya 43 : 10 , 13 ; 44 : 6 ; 48 : 12 ) Kukamba zoona , Aisiraeli anali ndi mwayi . 19 : 17 ) Zopeleka zaufulu zimathandiza pa nchito yofalitsa mabuku , ndiponso zimathandiza pa nchito yolalikila m’maiko osauka , kumene nchito yathu ikupita patsogolo kwambili . Atalandila mayankho , anaganizilapo mwakuya ndipo anaona kuti dziko la Taiwan lingakhale bwino kutumikilako . Kuwonjezela apo , dzina la Mulungu silinali kukhudzidwa , cifukwa Neko sanali kutonza Yehova kapena anthu ake . N’ciani cinamuthandiza kusintha maganizo ? ( 2 Pet . 3 : 15 ) Ngakhale kuti zinthu zopanda cilungamo zimene Petulo anacita zinawapweteka mtima Akhristu amitundu ina a mumpingowo , Yesu , mutu wa mpingo , anapitiliza kumugwilitsila nchito . ( Aef . 11 : 18 . Kuona zimene zili papepala kungawathandize kudziŵa mavuto ao ndi kuwathandiza kudziŵa zimene angacite ndi mavutowo . 5 : 29 ) Kodi tikuona mfundo yanji pamenepa ? Kodi Dzina la Buku la M’Baibulo , Lakuti Chivumbulutso , Limatanthauza Chiyani ? Kodi atumwi analimbikitsa bwanji Akhristu anzawo ? Koma ena amaona kuti cimalemekeza ulamulilo wa mphamvu wa Roma . Ndipo enanso amaona kuti ni cikumbutso ca kugwa kwa Yerusalemu na kacisi wake . Tikapemphela m’pamene anali kukhala womasuka kudya . ( Yoh . 16 : 13 ) Akhiristu odzozedwa onse analandila mzimu woyela , koma mzimuwo unathandiza kwambili atumwi ndi akulu ku Yerusalemu kuti akwanilitse udindo wawo monga oyang’anila . ( a ) Kodi Woweluza Yefita na Hana anali kulingana m’mbali ziti ? Munthu waumbombo amacita zinthu mopitilila malile , ndipo amacita kunyanya ndi khalidwe lake . Paulo anakumana ndi mavuto ambili , koma Yehova anamupatsa mphamvu kuti apilile . Mpingo wa ku Efeso utakhazikitsidwa , mtumwi Paulo analembela kalata Akristu a kumeneko . Ngati sitisamala tingayambe kumvetsela malangizo oipa a Satana , m’malo momvetsela malangizo acikondi a Mulungu . Imeneyi inali yofiila ngati moto . Wokwelapo wake analoledwa kucotsa mtendele padziko lapansi , kuti anthu aphane . ( 4 ) Kukhala oleza mtima ndi odalila pemphelo . Tifunika kutsatila malangizo omveka bwino amene mtumwi Paulo anapeleka kwa Akhristu a m’nthawi yake . Yehova anagonjetsa gulu la nkhondo la Sisera monga mmene Debora analoselela 11 , 12 . ( a ) Tingapindule bwanji ndi fanizo la khoka ? Ndipo munthu amene anathandizila Yehova kulenga anthu oyamba , sanaleke kukondwela ndi mbadwa za Adamu . ( Miy . Ine n’nauzidwa kuti nikatumikila ku Paraguay . Funso laciŵili n’lakuti , n’cifukwa ninji Yesu anatsiliza makambilano ake mwa kuchula Abulahamu , Isaki , ndi Yakobo amene adzaukitsidwa padziko lapansi ? M’maŵa tsiku lotsatila , asilikali ananilamulanso kuti nivale unifomu yausilikali . N’ciani cingathandize makolo acikhristu kuti akwanitse kuphunzitsa ana awo kukhala atumiki a Yehova ? Koma kupanga zosankha pasadakhale kungathandize kusapanikizika kwambili umoyo ukasintha . — Miy . Ni mmene zililinso masiku ano . — w17.02 , mapeji 26 - 28 . Kenako , onse aŵili anayamba kuphunzila Baibo na Mboni za Yehova . ‘ Chimo ’ limene Yesu anachula palembali silitanthauza mkangano waung’ono wapakati pa Akristu . Yesu anati : “ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” ( Ŵelengani 1 Timoteyo 4 : 12 - 16 . ) 4 : 22 ) M’malomwake , anawalimbikitsa kukonda anthu onse monga anansi ao . — Luka 10 : 27 . Ubwenzi wa Marilyn ndi Yehova ndiponso ndi mwamuna wake unasokonezeka . Kodi cikwati ca Mwanawankhosa cidzabweletsa madalitso otani ? Nanga Kristu adzakhala tate wa ndani mu Ulamulilo wake wa Zaka 1,000 ? 146 : 3 . Ndinali kungokhalila kudya , kugona komanso kukhala ndi moyo ngati wa Bruce Lee , Mchaina wa ku America amene anali katswili pa masewela a zibakela . ( Aroma 8 : 25 ) Sankhani Malemba amene amakamba zinthu zimene mumalakalaka kudzasangalala nazo m’dziko latsopano , ndipo muziyelekezela kuti muli kale m’menemo . Buku yochedwa New Catholic Encyclopedia , inakamba kuti kukondwelela Khrisimasi kunachulidwa koyamba “ mu kalenda ya zaka yaciroma yokonzedwa ndi Philocalus . Kalenda imeneyo ionetsa zocitika zoyambila mu 336 [ C.E . ] . ” Mkhristu winanso anakamba kuti pamene mkazi wake anamwalila mwadzidzidzi , anamvela “ ululu wosaneneka . ” 2 : 7 - 9 ; Luka 3 : 38 ) Ndipo udindo waukulu umene Mulungu anawapatsa unali umboni wakuti io anali ndi tsogolo labwino . Mwa kugwilitsila nchito mitanda isanu ya mkate ndi nsomba ziŵili , Yesu anadyetsa amuna pafupifupi 5,000 , osaŵelengela akazi ndi ana . Kodi Petulo anali munthu wotani ? Monga Paulo , mwina inunso zinakucitikilamponi kuti ngakhale munapanga cosankha motsatila citsogozo ca mzimu woyela wa Mulungu , zinthu sizinacitike monga mmene munali kuyembekezela . Lemba la Machitidwe 17 : 16 limati , pamene Paulo anali ku Atene , ‘ mtima unamuwawa kwambili poona kuti mumzindawo munali modzala mafano . ’ 8 Cikwati — Ciyambi na Cifuno Cake N’cifukwa ciani Abulahamu anapempha mkazi wake kuti akambe kuti iye anali mlongosi wake ? ‘ Mudzaona kusiyana pakati pa munthu wolungama ndi woipa . ’ — MAL . Koma Petulo analangiza Akhristu kuti : “ Lemekezani anthu , kaya akhale amtundu wotani . Kondani gulu lonse la abale . ” ( 1 Pet . Mukaunika pansi , mukwanitsa kuona bwino - bwino zimene zili pafupi . Ngakhale kuti ndife opanda ungwilo , tingam’kondweletse ngati tipitiliza kusintha umunthu wathu ndi kucita zimene amatiphunzitsa kudzela m’Baibulo . Mofulumila , tinaika mipando ku citseko na kuyamba kulongedza zovala . Jason , Cesar , ndi William Mu 2004 , Bungwe Lolamulila linakonza zakuti Baibulo la Dziko Latsopano limasulilidwe m’zinenelo zambili . Izi zimathandiza kuti anthu m’banja azikondana kwambili ndipo mipingo imakhala yogwilizana . — Akol . Zimene wamasalimo anauzilidwa kulemba pa Salimo 119 , zimatithandiza kumvetsetsa tanthauzo la kukonda coonadi ca m’Baibo . Iwo anali acangu pa nchito yolalikila . Mulungu anapeleka lamuloli kwa anthu pofuna kuwapatsa mwayi wom’thandiza pokwanilitsa colinga cake copanga dziko lapansi kukhala paladaiso , kuti anthu angwilo akhalemo kwamuyaya . Nanga mucita bwanji tsopano ? monga n’nakambila kumayambililo kwa nkhaniyi . Olo kuti anali atacita chimo , Aisiraeli ayenela kuti anali kuganiza kuti akali ku mbali ya Yehova . Izi zionekela bwino pa zimene Aroni anakamba . Baibulo limati : ‘ [ Mulungu ] wakhazikitsa dziko lapansi pamaziko olimba . Silidzagwedezeka mpaka kalekale , mpaka muyaya . ’ Olo kuti anthu a kumeneko anali aciwawa kwambili , Yehova anauza Yona kuti : “ Kodi ine sindikuyenela kumvela cisoni mzinda waukulu wa Nineve , mmene muli anthu oposa 120,000 , omwe sadziŵa kusiyanitsa dzanja lawo lamanja ndi lamanzele ? ” PAMENE Ophunzila Baibulo * anayamba kulalikila uthenga wabwino zaka zoposa 130 zapitazo , io anakumana ndi mavuto ambili . Anamucitila cifundo m’njila yakuti Ahabu sanaone banja lake lonse likuonongedwa cimene cikanakhala cinthu copweteka mtima kwambili . Masiku ano , ambili mwa ophunzila a Yesu oposa 8 miliyoni si odzozedwa . Nkhani yofotokoza za kulengedwa kwa zinthu imene ili m’buku la Genesis imamaliza ndi mau akuti : “ Mulungu anaona kuti zonse zimene anapanga zinali zabwino kwambili . ” 2 : 6 ) Mogwilizana ndi mau amenewa , Mulungu anaukitsa mnyamata wa ku Sunemu , kutsimikizila kuti alidi na mphamvu zoukitsa akufa . Mofanana ndi zinthu zina zambili , mkate tingaziuona monga ndi cinthu cosafunika kwambili . Onani nkhani yakuti , “ Umboni Woonetsa Kuti Maulosi a M’Baibo Ni Azoona . ” Komabe , iye anali mlaliki wopambana . * Ndiyeno ife tingacite bwino kudzifunsa kuti , ‘ Ngati zinthu zopanda cilungamo zaconco zanicitikila , kodi inenso ningakhale wokhulupilika kwa Mulungu ? Ena amanena kuti inapha anthu pafupi - fupi 10 miliyoni ndi kuvulaza ena 20 miliyoni . Kulimbikitsa ena sikulila zambili . Mwina mungangomwetulila popatsa moni munthu . Kunena zoona , nthawi zina zinali kuoneka ngati tiphedwa . 38 : 9 - 20 ) Conco , tengelani citsanzo ca atumiki okhulupilika amene anali ndi mzimu woyamikila . Koma kuwonjezela pa zonsezi , valani cikondi , pakuti cimagwilizanitsa anthu mwamphamvu kwambili kuposa cinthu cina ciliconse . ” — Akol . Ngakhale kuti sindinali kumva cinenelo cimeneco , ndinalimbikitsidwa kuyamba umishonale , kuphunzila cinenelo cina , ndiponso kukamba nkhani zolimbikitsa . Iwo ndi otangwanika kwambili ndi moyo wao ndi zocita zao cakuti amalephela kuona umboni wooneka bwino wosonyeza kuti Kristu wakhala akulamulila kuyambila 1914 , ndi kuti posacedwapa adzaononga dziko loipali . Monga munthu wa cikhulupililo , Inoki ayenela kuti anaona kuti ali yekha - yekha m’dziko la anthu osowa cikhulupililo . Kuti muone zitsanzo za milandu imene yatiyendela bwino m’maiko osiyana - siyana , onani Nsanja ya Olonda ya December 1 , 1998 tsamba 19 mpaka 22 . [ Mau okopa papeji 12 ] Kudalila kwambili Yehova kungatithandizenso tikakumana ndi mavuto aakulu . Ndithudi , anthu osadziletsa adzibweletsela mavuto ndi kubweletsanso mavuto kwa ena . 34 : 9 ) Mukamatumikila Yehova ndi mtima wonse , iye sadzalephela kukudalitsani . 27 : 11 . Ngati n’conco , tingayambe kukaikila kuti mapeto ali pafupi . Kodi mumadziona kuti muli m’Paladaiso ? Yehova anati : “ Mbeu ya mkaziyo idzaphwanya mutu wako [ Satana ] , ndipo iwe udzaivulaza cidendene . ” Ndi kuti kumene ndimakambilana ndi anthu ? Khalani ndi cidalilo cakuti Yehova adzakupatsani mphamvu kuti mugonjetse cizoloŵezi cokoka fodya . — Afilipi 4 : 13 [ Mau apansi ] Conco , anthu a Mulungu anauzidwa pasadakhale zimene zinali kudzawacitikila mtsogolo . Khalani m’malo anu , imani cilili ndi kuona Yehova akukupulumutsani . 6 : 8 - 10 ) Yesaya anavomela udindo umene Mulungu anam’patsa . Janet anati : “ Ndimatonthozedwa kwambili kudziŵa kuti Mulungu ndi ‘ tate wa ana amasiye ndi woweluzila akazi amasiye milandu . ’ Anali kudziŵanso zimene Ayudawo anapangana , zakuti munthu aliyense wovomeleza kuti amakhulupilila Yesu , adzamucotsa m’sunagoge . ( Yoh . Njila imodzi imene tingaonetsele kukhulupilika na cuma cathu ni mwa kupeleka ndalama zothandizila pa nchito yolalikila padziko lonse , imene Yesu anakamba kuti idzacitika . ( Mat . Kodi nipitiliza kutumikila Yehova na mtima wonse ? Ngakhale kuti Lefèvre anamwalila ali Mkatolika , zimene analemba zinathandiza kwambili pa nchito yomasulila Baibo . Zinacititsanso kuti anthu ayambe kutsutsa ziphunzitso za chechi ya Katolika . ( b ) abale ndi alongo athu ? AKHRISTU a m’zaka 100 zoyambilila anayesetsa kulalikila “ uthenga wabwino . . . wa Ufumu ” kwa anthu ambili . ( Mat . Masiku ano , ku Japan kuli ofalitsa 216,000 ndipo pafupifupi hafu ya io ndi apainiya . Lembani mndandanda wa zolinga zimene mungafune kuzikwanilitsa motsatila kufunika kwake . Zina mungaziike pa malo oyamba , aciŵili , acitatu mpaka conco . Anali kuwaphunzitsanso za nsembe ya dipo la Khristu Yesu , imene ili na phindu lalikulu ngako kwa anthu . Tingapindule bwanji ndi fanizo la khoka ? Kodi mungakonzekele bwanji ? Tingacite ciani kuti tikapindule ndi tsogolo labwino limene Mulungu watilonjeza ? Conco , ngati ana sadziŵa cikhalidwe ca makolo , sangafunenso kuphunzila cinenelo cawo ndi zikhulupililo zawo . 18 : 1 - 6 . Zimene ndinaona pakati pa Mboni , zinandidabwitsa kwambili cifukwa io analibe tsankho . Ndinakhala ndi cikumbumtima cabwino . ” ​ — JEFFERY 18 : 37 ) Komabe , kukhala wokhulupilika ku ziphunzitso za Khristu kungakhale kovuta ngati mnzathu wapamtima kapena m’bululu wathu amakana coonadi . N’cifukwa ciani Yesu sanatengemo mbali m’zocitika za m’dziko ? Komabe , sikuti tifunika kuonetsa cifundo nthawi zonse . Kuwonjezela pa Aisiraeli opanduka , n’ndani ena anatengeledwa ku ukapolo ku Babulo ? Nanga n’cifukwa ciani zinali zosatheka kutsatila malamulo onse a m’Cilamulo ? Baibulo lingakuthandizeni kupemphela kuti mukhale paubwenzi wabwino ndi Mulungu , osati kupemphela pofuna kutonthozedwa cabe . Elias Hutter na ma Baibo Ake a Ciheberi , Na . Kodi wolemba Salimo 102 anakumana ndi mavuto otani ? Mwina ndiye cifukwa cake Danieli , Yeremiya , ndi Ezara analemba mbali zina za Baibulo m’Ciaramu . * MLENGI wathu anatilemekeza kwambili mwa kutipatsa mphatso yamtengo wapatali ya ufulu wodzisankhila zocita . NYIMBO : 33 , 137 Izi tingaziyelekezele ndi mavuto amene Akristu amakumana nao masiku ano . ( Malaki 2 : 1 , 2 ) N’zoonekelatu kuti ngati sitimvela Yehova kapena tinyalanyaza uphungu wake tidzaononga ubwenzi wathu ndi iye . Woyang’anila ndendeyo anati : “ Ndicite ciani kuti ndipulumuke ? ” 55 : 22 ; Miy . Mukamva mau akuti “ Mapeto ali pafupi , ” kodi mumaganiza za ciani ? Kukhala ndi mzimu wotelo kudzatithandiza kucita zinthu mogwilizana tikadzakumana ndi mavuto kapena tikadzaletsedwa kugwilizana ndi abale athu a m’maiko ena . ‘ MUSAMACITE ZINTHU MOPITILILA MALILE . ’ Herodotus , katswili wacigiriki wolemba mbili yakale wa m’zaka za m’ma 400 B.C.E . , anakamba kuti Aiguputo ndiwo anali “ anthu oyamba kuikila kumbuyo ciphunzitso cakuti mzimu wa munthu sukufa . ” Adani amenewo anafunsa Yesu kuti : “ N’cifukwa ciyani ophunzila anu satsatila miyambo ya makolo , koma amadya cakudya ndi manja oipitsidwa ? ” Caciŵili , sitiyenela kudabwa masiku ano ngati ena ayamba kutsutsa otsogolela mumpingo . Sisera , wopondeleza wamkulu wa adani a anthu a Mulungu , anathaŵa wapansi kucoka kumalo omenyela nkhondo . Kusinkhasinkha pa zinthu zabwino zimene Yehova waticitila , kudzatithandiza kumuyamikila m’pemphelo . ( Sal . ( Machitidwe 20 : 35 ) Anthu opatsa amakhala acimwemwe cifukwa amapangitsa ena kukhala acimwemwe , ngakhale kuti angoŵapatsa nthawi cabe kapena kuŵacitila zinthu zina zocepa . Nanga bwanji za matenda ? Kuti mudziŵe zambili , onani nkhani 4 ndi 5 m’buku ili , Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova Iye ‘ akuyembekezela ’ moleza mtima nthawi pamene dzina lake lidzayeletsedwa mokwanila . Adamu ndi Hava atacimwa ndi kucotsedwa m’Paladaiso , Mulungu “ anaika akerubi kum’maŵa kwa munda wa Edeniwo . Anaikanso lupanga loyaka moto , limene linali kuzungulila mosalekeza , kuchinga njila yopita ku mtengo wa moyo . ” ( Gen . Abale ndi alongo athu amacoka ku malo osiyanasiyana , amakamba zitundu zosiyanasiyana , ndipo zikhalidwe zawo n’zosiyanasiyana . Mwadzidzidzi , muona kuti munthu akukulondolani kumbuyo kwanu . Polankhula ndi okhulupilila anzathu , tiyenela kugwilitsila nchito mau olimbikitsa osati ofooketsa . Kulela ana . ( Aroma 15 : 13 ) Ciyembekezo cimene Mulungu watipatsa cimatithandiza kupilila mayeso . Davide anacondelela Yehova kuti : “ Musanditaye nthawi ya ukalamba wanga . Musandisiye pa nthawi imene mphamvu zanga zikutha . ” — Sal . M’zaka za m’ma 400 B.C.E . , asayansi acigiriki anakamba kuti dziko ni lozungulila . Mphatso Yoposa Zonse , Na . Komabe , munthu wina angafunse kuti : ‘ Kodi zimene nimacita n’zofunikadi kwa Mulungu ? Lemba la Miyambo 18 : 13 limati : “ Munthu aliyense woyankhila nkhani asanaimvetsetse n’ngopusa , ndipo amacita manyazi . ” M’zaka zoposa 10 zapitazi , ofalitsa na apainiya opitilila 70 ocokela m’maiko 11 * akhala akubwela kudzatumikila m’dziko la mu Africa limeneli , limene muli anthu acidwi , ndipo ambili amalemekeza Baibo . Izi zinacitika zaka zingapo ine nisanabadwe . Lili ndi madzi oculuka amene ndi ofunika ku moyo . 5 / 1 Cigawo coyamba cili na mabuku 39 , ndipo muli “ mawu opatulika a Mulungu . ” Conco , zimenezi zinathandiza kuti mpingo usakhale ndi mtolo . Koma funso n’lakuti , Kodi imfa ya Yesu imacititsa bwanji kuti zikhale zotheka anthu kukapeza moyo wamuyaya ? Tumapepala twauthenga tungatithandize kuyambitsa maphunzilo a Baibulo . Koma popeza kuti ndico cinali cakudya patsikulo , ndinagula yogatiyo ndipo ndi imene tinagonela . Masiku ano , khalidwe la tsankho lili paliponse . Ni okonzeka ngakhale kufelana . ” M’nkhani ziŵilizi , tidzaphunzila mmene Khristu anaphunzitsila otsatila ake kuti akhale ogwilizana na kupewa tsankho limene limagaŵanitsa anthu . Malotowo anali maulosi ndipo Mulungu anafuna kuti Yosefe apeleke uthenga umene unali mu maloto amenewo . Mungayende naye muulaliki ndi kuona zimene mungaphunzile kwa iye . Koma mwanayo akayamba kudziŵa , kholo mosamala limayamba kumutailila pang’ono - pang’ono . Kodi ana angatonthoze bwanji ndi kulimbikitsa ena m’banja ? Ndipo kukhululukila ena n’kofunika kwambili kuti tilimbikitse mgwilizano mumpingo . 5 : 17 ; Aroma 12 : 12 ) Kukamba na Mulungu m’pemphelo n’kofunika kwambili kuti munthu akhale naye pa ubale wolimba . Koma monga mmene ndinali ndakambila , simungathe kumvetsetsa zinthu zonsezi pa nthawi imodzi . Koma m’Mabaibo ena , mau amenewa anawamasulila kuti “ helo . ” Timamvela monga mmene Debora na Baraki anamvelela pamene anaimba kuti : “ Inu Yehova , adani anu onse afafanizidwe cimodzimodzi , ndipo okukondani inu akhale amphamvu ngati mmene dzuŵa limakhalila . ” ( Ower . Mose anali kukonda kuyang’ana kwa Yehova kuti am’patse malangizo . N’nabadwa mu 1937 , ku mafamu a kufupi na mzinda wa Tokmok m’dziko la Kyrgyzstan . Posapita nthawi , vaagalu vinatizungulila ndipo vinali kutiuwa . Koma cifukwa cokhala ndi mzimu wosafuna kuuzidwa zocita , zinandivuta kugwilizana ndi banja langa . “ Lelo sinimvela bwino . 10 , 11 . ( a ) Kodi makolo ena amakhala na maganizo otani ? 45 : 5 - 9 . ( Sal . 147 : 6b ) Mau amenewa ni amphamvu kwambili . ( 1 Mafumu 18 : 22 - 45 ) Ahabu anaona zozizwitsa zimenezi , koma sanakhulupilile kuti zinatheka cifukwa ca mphamvu za Yehova . Yesu anali kudziŵa kuti ngati Atate wake amasamalila mbalame , sangakangiwe kusamalila anthu . ( 1 Pet . Izi ziyenela kuonjezela cikhulupililo cathu kuti kwangotsala kanthawi kocepa cabe kuti Mfumu ya Ufumu wa Mulungu iononge anthu oipa ndi kubweletsa dziko latsopano lolungama . — 2 Pet . Pali malemba ena amene anthu sangawamvetsetse mpaka nthawi yoyenelela itakwana . Koma akayanganuka kapena kuti kukololoka , sakhalanso woseka - seka ndipo amabwelelanso ku umoyo wake wodzala na mavuto na cisoni . ELIYA anali kuyenda m’cigwa ca Yorodano . Yesu anali kukonda kwambili kacisi wa Yehova ku Yerusalemu . Ndiye cifukwa cake ponena za Yesu , wolemba uthenga wabwino wina anagwilitsila nchito mau aulosi akuti : “ Kudzipeleka kwambili panyumba yanu kudzandidya . ” ( Sal . Iwo amayesetsa kukhalabe okhulupilika m’dzikoli , limene limalimbikitsa anthu kusalemekeza mfundo za Yehova . Ndiyeno , yesetsani kucita zinthu mogwilizana na mapemphelo anu , mwina mwa kucepetsako utali wa nthawi yophunzila . Kodi Ufumu wa Mulungu N’ciani ? Mogwilizana ndi pemphelo limeneli , tifunika kuyesetsa kuyeletsa dzina la Yehova . Ndinali kugwada pamanda a atate anga ndi kupemphela kuti : “ Conde Mulungu , ndiuzeni kumene kuli atate . ” Kodi inu mumaona nchito yolalikila kukhala yofunika pa umoyo wanu mwa kupatula nthawi yopita mu ulaliki wiki iliyonse ? Kodi tiyenela kukhala ndi zolinga ziti polalikila ndi mtima wathunthu ? Ngati siticita zimenezi , iwo adzaphunzila kubisa zolakwa zawo . ” — Robin . Mayankho anu pa mafunsowa adzaonetsa ngati inu , mofanana ndi Nowa , ‘ mumayenda ndi Mulungu woona ’ kapena ai . ( Yobu 23 : 12 ) Yobu iye mwini anakamba kuti anamvapo za Mulungu . Kuwonjezela apo , ngati ndise opatsa , timakhala acimwemwe cifukwa “ kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” Akhristu apaulendo ayenela kuti anali kukonda kugona ku nyumba za okhulupilila anzawo . Kodi cidziŵitso , kumvetsa zinthu , na nzelu zimasiyana bwanji ? MBILI : WOKWIYA MSANGA NDI WACIWAWA Amuna amene anali kudzakwatila ana ake anaona ngati Loti anali ‘ kunena zoceza . ’ KODI AKUFA ADZAUKA LITI ? Kodi kuuka kwa olungama ndi osalungama kudzacitika liti ? N’nali kukumbukila mwamsanga uyo anali kuseli kwa zithunzi zonyansazo . Kodi umoyo wa anthu a m’banja limodzi umasiyana bwanji ? Nanga timaphunzila coonadi m’njila zosiyana - siyana ziti ? ( b ) Kodi mmishonale wina amathandiza bwanji abale acicepele ? ( Genesis 13 : 1 , 2 , 5 - 9 ) Cimeneci ndi citsanzo cabwino cimene tiyenela kutengela . N’zodziŵikilatu kuti iwo anamva kuti Yehova anali kufuna anthu odzipeleka kuti akamenye nkhondo . “ Nchito yapadelayi inanithandiza ngako pa utumiki wanga . Nkhani yoyamba pa nkhani ziŵili izi idzafotokoza mmene tingakhalile odzicepetsa ndi acifundo monga Yesu . Mbali yoyamba , mau a m’Baibulo ndi osavuta , acindunji , ndiponso osangalatsa . N’zoona kuti mavuto anu angakhale osiyana ndi a mlongo Bianca ndi a m’bale Paula . Rose anakamba kuti : “ N’nabadwa na matenda osacilitsika , amene amacititsa kuti nthawi zonse nizimvela kuŵaŵa maningi . Lamulo lakuti tizikonda anzathu mmene timadzikondela limachedwa “ lamulo lacifumu . ” Nkhaniyo imati , “ nthawi yomweyo anthuwo anacoka . ” ( Num . Ineyo ndi mwamuna wanga tikucita upainiya . Ndiye Amacititsa Mavuto ? Koma sanapeze pulaneti lina limene lili ndi zinthu zonse zimene anthu amafunikila kuti akhalebe ndi moyo . Zakalezo zapita . ’ ” — Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . ( Mungapeze mfundo zina zothandiza m’buku la Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu , phunzilo 21 mpaka 23 . ) Ndiyeno , madziwo anayambanso kugawanika . — 2 Maf . Koma n’cifukwa ciani kudzicepetsa kuli kofunikabe ? Komabe , amacititsa anthu ambili m’dzikoli kukhala ndi mtima woipa ngati wake . ( Sal . 72 : 8 ) Zozizwitsa za Yesu zimatsimikizila kuti iye amafunitsitsa kugwilitsila nchito mphamvu zake kuthetsa mavuto amene tikukumana nao , ndipo posacedwapa adzacita zimenezo . Inde , pemphelo la citsanzo limatitsimikizila kuti palibiletu cingalepheletse cifunilo ca Mulungu kucitika . — Sal . Sauli anauza Davide kuti : “ Sungapite kukamenyana ndi Mfilisiti ameneyu , cifukwa ndiwe mwana , ndipo Mfilisiti ameneyu wakhala akumenya nkhondo kuyambila ubwana wake . ” Yobu anaphunzila coonadi ca mtengo wapatali cimeneci , koma Baibo siikamba mmene anaciphunzilila . Iwo anati : “ Taona kale mmene Yehova wasamalila zosoŵa zathu zakuthupi . ( Genesis 32 : 22 - 31 ) Patapita nthawi , Yosefe anadziŵa kuti ana a Isiraeli adzakhala tate wa mafuko a mtunduwo ! Adamu anacimwa , ndiye cifukwa cake anafa . M’bale Nathan Knorr na Frederick Franz , ocokela ku likulu , anabwela ku Portugal kudzasangalala limodzi nafe pa msonkhano wosaiŵalika ku Oporto ndi ku Lisbon . Anthu 46,870 anapezekapo . Nikotini amacititsa kuti munthu avutike kwambili kuti aleke kukoka . ( Aefeso 6 : 16 ) Ndiponso cifukwa cokhulupilila Yehova , sitimada nkhawa kwambili tikakumana ndi mavuto . 8 : 14 ; Agal . 2 : 9 ) Cotelo , n’zotheka Akhristu amene ni osiyana zibadwa kutumikila pamodzi masiku ano . Kodi mumakhululukila ena mwamsanga ? Kodi angacite ciani ngati akuona kuti umoyo wa m’cikwati ni wovuta kwambili kuposa mmene anali kuganizila ? 3 : 1 - 4 ) M’Baibo muli zitsanzo za anthu auzimu komanso za anthu akuthupi . ( Ŵelengani 1 Akorinto 10 : 24 . ) Ena anaphunzila coonadi pambuyo pokwatilana , koma mnzawo sanafune kukhala Mboni . Kwa anthu okana malangizo ake , Yehova anati : “ Munasankha zinthu zimene sindisangalala nazo . . . . Tikamaŵelenga nkhani zimenezi , timadziŵa mavuto amene acinyamata amakumana nao , ndipo timadziŵa mmene tingawathandizile ndi kuwalimbikitsa . Aliyense wa ife ayenela kumvela cenjezo la Inoki na kucenjezako ena . ( Aroma 12 : 18 ) Monga otsatila a Khristu , tiyenela kuyesetsa ‘ kukhala mwamtendele ndi anthu onse . ’ Panthawi imeneyo , Yehova adzapitiliza kutiumba ndi kutiphunzitsa m’njila imene sitinaganizilepo . Nyumbayi inali pa malo okwana mayeka aŵili na hafu , ndipo panali mitengo ikulu - ikulu . Funa - funani Ufumu coyamba ndi cilungamo cake . A Zulu : Tiyambe ndi kufotokoza mwacidule zimene Mfumu Nebukadinezara inaona m’loto lake . Conco , ufulu umene anthu na angelo ali nawo uli na malile . Kupilila kumatithandiza kukhala olimba mtima , okhulupilika , ndi oleza mtima . M’baleyo anafunsa kuti , “ Kodi zonse zili bwino M’bale Herd ? ” ( Ezekieli 18 : 2 , 3 ) Koma kodi zimenezo n’zoona ? Mau a Mulungu anatsogolela amuna omuimilako . Munthu wina wosaona anati : “ Mphamvu yoona si ili m’maso koma ili m’maganizo . ” Mtundu wonse unali kudzachedwa ndi dzina lake ! Amafuna kudziŵa zimene zimawadetsa nkhawa cifukwa amawakonda . Yehova Amatitonthoza m’Masautso Athu Onse , June ( a ) Kodi anthu oipa akali na mwayi wotani ? Malinga ndi buku lakuti Vine’s Expository Dictionary of Old and New Testament Words , mau amene Yohane anagwilitsila nchito amatanthauza “ kudalila wina wake kapena cina cake , osati cabe kukhulupilila . ” Mwacitsanzo , ndani mwa anthu aŵiliwa amene mungalemekeze kwambili ? Tingaonetse bwanji kuti tili ndi cikhulupililo monga ca Yefita ndi mwana wake ? Conco anapitiliza kulambila Mulungu pa kacisi , ndi kum’condelela m’pemphelo . ( 1 Sam . 2 : 4 , 19 ) Tiyeni tipitilize kucita khama kuti tizicita zinthu mogwilizana ndi lonjezo lathu la kudzipeleka . Kuonjezela pamenepo , “ malemba oyela ” sanali ndi uthenga umodzi wa Mulungu . Anthu ambili amene anakulila m’mabanja ocita bwino , okhala ndi zinthu zambili zabwino , samaona kufunika kwa zinthuzo . Malamulo ocokela kwa Yehova ndi olungama , amasangalatsa mtima . Cilamulo ca Yehova ndi coyela , cimatsegula maso . ” Cakudya cakuuzimu cimene timalandila kudzela mwa kapolo ameneyu , cimatithandiza kulimbitsa cikhulupililo cathu . Koma kuonjezela pamenepo , anapezamonso zakudya zambili . ” 19 : 18 ; Aroma 12 : 17 - 21 ) Citsanzo ca Yosefe n’colimbikitsa kwa ife . Makolo amapatsa ana ao mphatso zabwino mwa kuwaphunzitsa kupemphela ndi kuwathandiza kuona Yehova monga Atate wakumwamba amene amatisamalila . CITSANZO CAKE : Yesu anapemphela mogwilizana ndi mmene anaphunzitsila ena kupemphela . Iye anapemphela kuti : “ Atate ndikukutamandani pamaso pa onse , inu Ambuye wakumwamba ndi dziko lapansi . ” Ngati mumakhala kutali ndi makolo anu , Mboni kapena munthu wina amene akhala pafupi ndi makolo anu angadziŵaonako ndi kukudziŵitsani mmene umoyo wao ulili . N’zoona kuti zolakwa zimasiyana kukula kwake , ndipo kwa ise anthu opanda ungwilo zolakwa zina n’zovuta kwambili kukhululukila . ( Salimo 104 : 33 ) Kodi inunso mumafuna kutamanda Mulungu ? Nawonso ophunzila a Yesu anayambukilidwa na khalidwe limeneli . Zimene Ena Amalosela Zimacitika , Koma Zambili Sizimacitika 3 Ndiponso tiyenela kuphunzila mmene Yesu anali kukambila ndi anthu kuti nafenso tizitha kukamba mau olimbikitsa ena . Baibulo la Dziko Latsopano , lathunthu kapena mbali yake , lipezeka m’zinenelo zoposa 150 . M’ma Baibo ena , liu limene linamasulidwa kuti “ zosathandiza , ” analimasulila kuti “ zacabecabe , ” “ zopanda phindu , ” na “ zotha nchito . ” Pambuyo pake , Petulo anayamba kugwilizana ndi Akhristu a mitundu ina komanso kudya nawo . Zimene siningakwanitse nimasiyila Yehova . ” Mu 1952 , ine na abale ena okwana 6 ocokela ku Philippines , tinasangalala kwambili kulandila ciitano cakuti tikaloŵe kilasi ya namba 20 ya Sukulu ya Giliyadi . Hana anakondwela kwambili . Cimatithandizanso kuti tizipemphela ndi kuimba nyimbo zotamanda Yehova . ( Chiv . 17 : 1 , 5 , 16 , 17 ; 19 : 1 , 2 ) Kenako pa Aramagedo , yomwe ndi “ nkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu Wamphamvuyonse , Kristu adzaononga mbali yonse yotsala ya dziko la Satanali . ” Kodi kutsogolo kudzacitika ciani cimene cikuonetsa kuti kuphunzitsa ena n’kofunika kwambili ? Anayamba kusamba , kudulila ndevu , ndi kuvala zovala zabwino zimene Don anam’patsa . Atapeza mpukutu wa Cilamulo ca Mose , kalembela wa Yosiya anayamba kumuŵelengela . Lembali limati : ‘ Musamade nkhawa ndi kanthu kalikonse , koma pa ciliconse , mwa pemphelo ndi pembedzelo , pamodzi ndi ciyamiko , zopempha zanu zidziŵike kwa Mulungu . Katswili wina wa zamaphunzilo wa m’zaka za m’ma 1900 , dzina lake Friedrich Nietzsche , anacha imodzi mwa nchito zake kuti Wokana Kristu . Conco , ndimapempha Yehova kuti andidalitse . ” Pamene anacotsapo civundikilo pa poto , anadabwa ataona kuti munali cabe supu ya chizi . Ndipo iye anawathandizadi , cifukwa Mulungu wathu “ amapeleka mphamvu kwa munthu wotopa . ” Niyamikila kwambili Yehova cifukwa conithandiza kumasuka ku khalidwe lodziwononga . Ayuda ambili m’nthawi ya Malaki sanali kumvela Yehova . Kucokela nthawi imeneyo , Reylene wakhala citsanzo cabwino pa nkhani yokhulupilila lonjezo la Yehova la pa Mateyu 6 : 33 , 34 . Tidziŵa bwanji zimenezi ? M’kupita kwa nthawi , Mboni za Yehova zinasintha kamvedwe kawo pankhani yosatengako mbali m’nkhondo . Anthu amene anakulila m’banja lopanda cikondi , amasangalala kukhala m’paradaiso wauzimu cifukwa abale ndi alongo amawakonda . “ Kuti makolo anu azikudalilani , njila yabwino ni kucita zinthu zoonetsa kuti ndimwe munthu wokhwima m’maganizo komanso wodalilika . Mungacite zimenezi osati cabe pamene makolo anu alipo koma olo pamene iwo palibe . ” — Sarahi . Maiko ambili anaona kuti nkhondo zinali kuthandiza kupeza akapolo m’njila yosavuta . ( Aroma 4 : 19 , 20 ) Nanga bwanji Sara ? Nthawi zambili , timakhala ndi Baibulo m’dzanja lathu kuti tiligwilitsile nchito . Tidzaphunzilanso mmene tingatengele citsanzo cawo m’dziko logaŵikanali . Kuonjezela apo , gulu lina lacitatu lofunika analicha kuti “ abale ” a Mfumu . — Ŵelengani Mateyu 25 : 31 - 46 . Patapita miyezi 6 , tinasamukila m’tauni ya Oswestry , m’dela la Shropshire , cifukwa tinali ndi mwai wocita lendi famu yathuyathu yaing’ono . Cinthu cimodzi cofunika cimene tingacite ndi kulimbikitsa ndi kuthandiza makolo na ana awo . Analinso kum’dziŵa bwino Yehova , ndipo izi zinam’limbikitsa kucita zinthu zoyenela . Nanga n’cifukwa ciani Paulo ananena kuti “ anamva mau osachulika , amene sikololeka munthu kuwanena ” ? Kwa zaka zambili , io anali kucita upainiya ndipo anali kutumikila kumalo amene kukufunika ofalitsa ambili m’dziko lao . 22 : 25 - 29 . Kodi woipayo anayamba bwanji kulamulila anthu ? ( Mika 7 : 7 ) Monga mmene Mika anacitila , nafenso tifunika ‘ kuyembekezela moleza mtima . ’ Komanso amakambilana ndi anthu amene ali pansi , amene nchito yawo ni kumuuza nthawi imene afunika kunyamuka , kumene afunika kupitila , na nthawi imene afunika kutela . 4 : 7 - 9 ; Agal . N’cifukwa ciani ino ndiyo nthawi yothandiza abale a Kristu ? Buku lina linakamba kuti asayansi apeza kuti tuzilombo twa thaifodi ndi tuzilombo twina toyambitsa matenda , tumafa mwamsanga akatusakaniza ndi vinyo . — The Origins and Ancient History of Wine . Mungakambilanenso mafanizo amene ali patsamba 10 mpaka 20 mu kabuku kakuti The Origin of Life — Five Questions Worth Asking . Inde akuigwila , ndipo masiku ano anthu ambili amva uthenga wabwino ndi kukhala ophunzila kuposa kale . Khalanibe ndi mtima wofuna kuphunzila . M’nkhani ino , tidzakambilana za kudzicepetsa ndi cifundo . Rabeka atamaliza kutunga madzi , mwamunayo anam’patsa mphatso za mtengo wapatali . Ndingatsimikize bwanji kuti adzasangalala ndi zosankha zanga ? ’ Kodi tidzamvela malangizo ndi kugwila nchitoyo mwakhama ndiponso mosangalala ? Koma kanathandiza kuti salimo yonse imeneyi izionetsa bwino ciyembekezo cimene atumiki a Yehova akhala naco kwa nthawi yaitali . Ciyembekezo cakuti Mulungu adzaononga oipa na kupatsa anthu olungama umoyo wamtendele ndi waulemelelo . — Sal . Mwina acibale anu amene munali kuyembekezela kuti akutonthozani , ndi amene akucititsa zinthu kukhala zovutilatu . Tingacite ciani kuti tithetse nkhaniyo na kubweza m’bale wathuyo ? Mofanana ndi m’bale ameneyu , nanunso Mulungu adzakulimbitsani mukafooka . Akelubi anaikidwa m’Malo Oyela Koposa ndipo ndi mkulu wa ansembe yekha amene anali kuwaona . Mosakaikila , Yesu ndi wokondwela kwambili ndi anchito ake . Kuyambila m’caka ca 1970 , nakhala na mwayi woyendela maofesi a nthambi osiyana - siyana a Watch Tower Society . N’nali kuyendela maofesi a nthambi angapo kwa mawiki ocepa m’caka ciliconse kapena pambuyo pa zaka ziŵili . Farao anacita cikondwelelo cokumbukila kubadwa kwake , comwe atumiki a Mulungu sacita . Kuonjezela apo , Adamu anataya moyo wangwilo ndipo mbadwa zake zinatengela kupanda ungwilo kumeneko . Uthenga wa Ufumu umatipatsa cimwemwe coculuka . N’ciani cingathandize makolo kuphunzitsa ana ao mwa kuuzimu ? 24 : 45 . Inalidi nthawi yosangalatsa kwambili . Tiyenela kulemekeza moyo na kuuona kukhala wamtengo wapatali . Koma m’bale mmodzi pa aŵiliwo anakhumudwa cifukwa ca mmene mlongoyo anam’patsila moni . Kodi tifunika kukhalabe conco n’kumangoyembekezela ? Makolo athu oyambilila anasankha kusamvela Mulungu . Nthawi zoposa 30 , timaŵelenga kuti malamulo a m’buku la Levitiko anacokela kwa Yehova . Izi n’zimene zinacitikila mlongo wina dzina lake Amy . Pokhala mbadwa za Adamu zopanda ungwilo , cibadwa cathu cimakhotelela pa kulakwitsa zinthu , kucita zoipa , na kucimwa . Cifukwa cakuti Ayuda anali kukhala m’madela ambili , anthu amene sanali Ayuda anayamba kudziŵa Malemba Aciheberi . Mungamuuzenso kuti mumakhulupilila Yesu Khristu , amene anafa monga nsembe ya dipo . Mayiyo anakamba kuti anali kufuna kudzipha masana omwewo , ndipo pamene Kenneth anatuma foni , apo n’kuti akulembela mwamuna wake kakalata komudziŵitsa kuti wadzipha . Koma n’zomvetsa cisoni kuti onsewa sanayamikile colowa ca Yosiya . Ngati papita nthawi itali kucokela pamene munakukila mu mpingo wina koma zikukuvutani kujaila , n’ciani cingakuthandizeni ? Koma kuwonjezela pa zonsezi , valani cikondi , pakuti cimagwilizanitsa anthu mwamphamvu kwambili kuposa cinthu cina ciliconse . ” 4 : 9 ) Liu la Cigiriki lomasulidwa kuti “ kuceleza ” limatanthauza “ kukonda alendo kapena kuwakomela mtima . ” Yesu anali kudziŵa bwino kuti n’zosavuta kwa anthu opanda ungwilo kugonja cifukwa ca zofooka za thupi . Pa ulendo umenewu McCartney ananidziŵikitsa kwa mtsikana wina wauzimu , Bethel Crane . Cifukwa ca mikangano imene inalipo , Nsanja imeneyo inati : “ Nchito ya Ufumu yabwelela m’mbuyo makamaka m’maiko a Germany ndi France . ” 6 : 16 ) A khamu lalikulu naonso ali ndi dzina lopatsidwa ndi Mulungu lakuti Mboni za Yehova . Timayamikila kwambili kuti Yehova anasunga “ zinthu zonse zimene zinalembedwa kalekale , ” kuti tikhale ndi “ ciyembekezo cifukwa malembawa amatithandiza kupilila ndiponso amatilimbikitsa . ” Iye anakambanso kuti : “ Tinapatsana manamba ya foni n’colinga cakuti azitiitanako pakakhala zocitika zauzimu kapena zina . ” Anthu ambili amene ndinali kuvina nao anali kucita ciwelewele , kusuta fodya , ndi kuledzela , ndipo ine ndinali kudalila zithumwa za mwai mofanana ndi ovina ena . A m’banja langa ataona zimenezi , anacita mantha kuti hosiyo idzanivulaza . ( Yakobo 2 : 17 ) Zocita zanu n’zimene zimaonetsa kuti muli ndi cikhulupililo colimba . Tikamva maganizo ake , tingadziŵe mmene tingam’thandizile kuti adziŵe zimene Baibulo limanena pankhani ya helo . Ngati ndife okoma mtima ndi oganizila ena , tidzaonetsa kuwala kwathu , tidzaonetsa kuti timatsatila mfundo za m’Baibulo , ndi kuti timalemekeza atate wathu wakumwamba . ( Mat . ( a ) Kodi mlongo wina anakhudzidwa bwanji na malemba amene anagwilitsidwa nchito pa msonkhano ? Ndiyeno Mulungu anati citsa cake cisiidwe m’nthaka . Kodi n’kulakwa kulanga ana anu ? Yehova akanalanga Aroni nthawi imeneyo cifukwa ca zolakwa zimenezi . Koma buku limeneli ndi lokayikitsa ndipo amene analemba sadziŵika , ngakhale kuti ena amanama kuti linalembedwa ndi Inoki . Motelo , tiyenela kusankha amene tidzamvela . Amene adzapulumuka masiku otsiliza adzakhala m’paradaiso padziko lapansi N’naona monga kuti zikucitikila munthu wina osati ise . Kazuhiro na mkazi wake , Mari , anagulitsa mamotoka awo , anapeza mapasipoti , na kugula matiketi a ndeke . Mu 1914 , munthu wina wa ku America amene analoŵa nkhondo mwa kufuna kwake , analemba kuti : “ Ndine wokondwa kwambili cifukwa coganizila zinthu zosangalatsa zimene zidzacitika mtsogolomu . ” Iye amafuna kuti tileke kucilikiza ulamulilo Mulungu ndiponso kum’tumikila . Koma kwa ife sizili conco . Iye anali kusinkhasinkha zimene anaŵelenga m’Baibulo ndipo anacita khama kuti asinthe umunthu wake . Elizabeth anakamba kuti , “ Cikwati cikatha , munthu amafuna thandizo . Tiyeni tikambilane mbali zake zina zofunika . Yakobo anati : “ Akacokapo , nthawi yomweyo amaiŵala kuti ndi munthu wotani . ” Panthawiyo , sitidzakhalanso na nkhawa iliyonse . Conco tiyenela kuyesetsa kupewa kucita macimo aakulu kuti Mulungu azitikhululukila . Anthu ena amakamba kuti mumlalang’amba wathu , wochedwa Milky Way , muli nyenyezi mabiliyoni ambili . Iye anawayeletsa mwakuuzimu kuti utumiki wao kwa Yehova ukhale wovomelezeka . ( Yes . 4 : 2 , 3 ; Mal . Iwo ndiwo anali oyamba kupatsidwa “ mau opatulika a Mulungu . ” ▪ Tifunika Kukhala Oyela m’Makhalidwe Athu Onse Conco mmalo mokhumudwa poona kuti thandizo la anthu ndi losakwanila , muyenela kuona mavuto ngati mmene Paulo anawaonela . Muyenela kuwaona kuti ndi mwai wanu wosonyeza kuti mumakhupilila kwambili Yehova ndi kuyembekezela kuti iye adzakusamalilani mwacikondi . Ganizilani mmene mungayankhile mafunso awa : N’cifukwa ciani ndimakhulupilila kuti kuli Mulungu ? Petulo analemba kuti Yesu “ anaphedwa m’thupi , koma anaukitsidwa monga mzimu . ” Kodi Cilamulo ca Mulungu kwa Aisiraeli Cinali Colungama ndi Cosakondela ? — November - December N’ciani cinasintha pa nchito yolalikila ? Apa m’pamene n’nayambila kusiya zinthu zina kuti nitsatile Ambuye . Mlongo wina wacitsikana analemba kuti : “ Ndinamaliza kuŵelenga buku lonse la Uthenga Wabwino wa Mateyu panthawi imodzi . Yehova amatiuza kuti tidzazunzidwa m’njila zosiyanasiyana . Koma ngati mayeselo apitilizabe mungataye mtima . Rutherford , amene anali kuyang’anila nchito yolalikila pa dziko lonse . Koma mwapemphelo , Yehova anandithandiza kulimbana ndi zinthu zimene pandekha sindikanatha kulimbana nazo . Caciŵili , akulu amene amapenda ziyeneletso ndi kuika abale pa udindo amapempha mzimu wa Yehova kuti uwathandize kudziŵa ngati m’bale akukwanilitsa ziyeneletso za m’Malemba . Mtumwi Paulo alemba kuti : “ Abulahamu ataonetsa kuleza mtima , analandila lonjezo limeneli . ” Iŵili mwa mitsinjeyo ikudziŵika mpaka lelo . Woyamba ni Hidekeli , umene lomba umachedwa Tigris , ndipo waciŵili ni Firate . Nthawi zambili anthu opanda ungwilo amakonda kuyelekezela zinthu . Koma mau a Mulungu amatiuza kuti tiyenela kuika maganizo athu pa zimene timakwanitsa kucita . Ine ndi banja langa tinakakhala m’kampu ya othawa kwao imene inali kumadzulo kwa dziko la Mozambique mpaka kufika mu June 1974 . Akulu angacitenso bwino kuona ngati khadi yanu ya magazi ni yosainiwa bwino . Solomo anakonda “ akazi ambili acilendo ” cakuti anadzakhala ndi akazi 700 ndiponso 300 apambali . Amalangizidwa kuti kucita maphunzilo apamwamba kumatsegula mwayi wokapeza nchito yabwino komanso ya malipilo oculuka . Ndipo nthawi zambili amawaonetsa nkhani zofalitsidwa zoonetsa kuti anthu ophunzila ku mayunivesiti aconco , amalandila ndalama zambili kuposa amene sanapite ku univesiti . Robert , amene tam’chula kuciyambi kwa nkhani ino , anati : “ Pambuyo polimbitsa ubwenzi wanga na Yehova , n’nakhala mwamuna wabwino komanso tate wabwino . DZIKO : FRANCE Iye amaona kuti mapemphelo ake aŵili acindunji anayankhidwa . Kucita izi kumalimbikitsa mgwilizano . Kodi mwaona kuti Iye amakuumbani mosamala ? Mungacite ciani kuti mudzipeleka mphatso na colinga cabwino ? Panthawiyo , pa nthambi panali nchito yomanga . Conco , ananiitana kukathandiza , ndipo n’nakhala ciwalo ca banja la Beteli ku Canada pa December 1 . N’cifukwa ciani cikondi n’cofunika m’banja ? ( Yohane 17 : 3 ) Timacita zimenezo mwa kudziŵa maganizo a Mulungu kudzela m’Baibulo . Yesu anakambanso kuti : “ Pamenepo amene ali mu Yudeya adzayambe kuthaŵila kumapili , ndipo amene ali mkati mwa mzindawo adzatulukemo . Amene ali m’madela akumidzi asadzaloŵe mumzindawo . ” Zaka 8 zotsatilapo ndinali ndi mwai wocita upainiya ku Tasmania . Atumwi okhulupilika a Yesu nawonso anapeleka citsanzo cabwino kwambili ca kukhala olimba mtima . M’nkhani yokonkhapo , tidzakambilana zimene ifenso tingacite kuti tsankho lisasokoneze mgwilizano wathu . Conco , kaya mwana wanu ni wamng’ono kapena wosinkhukilako , musakangane naye pokambilana nkhani imeneyi . “ Nchitoyi Ndi Yaikulu ” ( zopeleka ) , Nov . Mboni zinakananso kutengako mbali pa nkhondo zimene zinacitika ku maiko a Balkans pamene ulamulilo wakale wa Yugoslavia unagwa . Mofananamo , coonadi cimene timaphunzila m’Mau a Mulungu cimatiteteza ku ziphunzitso zabodza zimene zikhoza kutiwononga mwauzimu . ( Yoh . Anthu ambili masiku onse amayamikila Mulungu cifukwa ca mphatso ya moyo . Iwo anali osiyana kwambili ndi anthu ena amene ndinali kukhala nao . Conco , Yehova anapanga mtundu watsopano wa otsatila a Kristu . Iwo anakhala gulu limene linali kuimila Yehova . Makolo — Ŵetani Ana Anu , 9 / 15 15 , 16 . ( a ) Kodi lemba la Yohane 13 : 34 , 35 , lionetsa kuti tili na udindo wanji ? 6 : 10 ; 9 : 2 ) Mkazi wacikulile wamasiye Anna “ sanali kusoŵa pakacisi . ” A Yohane : Inde , ndiganiza conco . Kodi Yehova anacita ciani ataona zinthu zopanda cilungamo zimenezi ? Mwacitsanzo , limafotokoza zimene Yosefe anacita atadziŵa kuti Mariya ali na pakati , zimene mngelo anamuuza pankhaniyi kupyolela m’maloto , ndi zimene iye anacita pomvela malangizo a mngeloyo . ( Mat . Ngakhale mutakonzekela , mwina mungakhalebe osamasuka kuuzako ena zikhulupililo zanu . Kuphunzila mwakhama Malemba kunam’thandiza kuzindikila kuti “ kuphunzila coonadi ca Mulungu pakokha . . . kumabweletsa cimwemwe cacikulu . ” Kodi atumiki a Mulungu aonetsa bwanji kuti amakondana ? Pamafunika khama kuti munthu apitilize kucita zinthu mogwilizana ndi kudzipeleka kwake . ( 2 Tim . 3 : 1 - 4 ) Kuwonjezela apo , ise Akhristu tili pa nkhondo yauzimu yolimbana ndi Satana na ziphunzitso zonama zimene amafalitsa . ( 2 Akor . Munazindikila kuti anthu ndi otalikilana ndi Mulungu . ( Akol . Iye anapatsa Adamu ndi Hava , malo okongola okhalamo , zonse zofunika paumoyo , ndi nchito yabwino ndi yokhutilitsa . Anati ni 1 Petulo 5 : 7 imene imati : ‘ Mutulileni nkhawa zanu zonse [ Mulungu ] , pakuti amakudelani nkhawa . ’ Yesu anapeleka malangizo amenewa pofuna kutiphunzitsa mmene tingathandizile Mkristu mnzathu mwacikondi . Komanso , muzifunsilako kwa Mkhristu wokhwima kuuzimu . Akapezeka pa nyumba , samafuna kumva uthenga wa Ufumu , m’malo mwake amakhala amphwayi , mwinanso ankhanza . 3 : 11 , 12 , 14 ) Inde , tiyeni tiyesetse kukhala oyela ndi kupitilizabe kucilikiza Mfumu Yamtendele . Iyo ndi yamphamvu ndipo ululu wake ndi waukulu kwambili . NYIMBO : 7 , 3 ( Mat . 25 : 21 , 23 ) Kodi mau amenewa siyakulimbikitsani kupitiliza kutumikila Yehova mokhulupilika ? 5 : 19 ) Komabe , n’zokondweletsa kudziŵa kuti Yehova ni “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse . ” Akhoza kukumana ndi mayeselo ngakhale panthawi yanchito . 3 : 9 . Nthawi na nthawi , tifunika kudzifunsa kuti : ‘ N’ciani cimene nimakonda maka - maka ? Pa May 20 , 2015 , mwamuna wanga amene n’nakhala naye m’cikwati zaka 66 , anamwalila . ( b ) Tingacite ciani ngati anthu ena atitamanda pa zabwino zimene tacita ? Ndipo akaidi onse maunyolo awo anamasuka . Conco , tiyenela kuyembekezela Yehova ndi kuona mmene adzayankhila mapemphelo athu . — Yelekezelani ndi Yesaya 29 : 16 ; 45 : 9 . Ŵelengani Afilipi 2 : 4 . Iye anali mkazi wauzimu , ndipo anali wamakhalidwe abwino . Moto tikaugwilitsila nchito bwino umakhala wothandidza . ( Agal . 6 : 15 , 16 ) Nsembe ya Yesu ndi imene inatheketsa zimenezi . Ganizilani kuti mukuona mwamuna wacikulile akuuza Rabeka lonjezo la Yehova kwa bwenzi Lake , Abulahamu , pamene akuotha moto usiku . Ofalitsa ena amene ayesa kutsatila malingalilo awa akhala osangalala ndi zotsatilapo zake . Kodi Solomo anam’kwiyitsa bwanji Yehova ? ▪ Awa Ndi Malo Athu Olambilila Zinthu zimene anthu anali kuona kuti n’zosayenela kupenyelela pa TV m’ma 1950 , masiku ano anthu ena amacita kuzionelela pamodzi monga banja pofuna kuonetsa kuti zilibe vuto . Inde , Davide anafunikadi mnzake weni - weni . Ngati tisinkhasinkha zimene Baibulo limanena ponena za mmene Yehova anacitila ndi atumiki ake okhulupilika akale , tidzaphunzila zinthu zambili zabwino za Mulungu . Ngakhale kuti tili m’nthawi yovuta kwambili , ndipo tikuona kuti vikwati vili kupasuka kulikonse , n’zotheka kuti ife tikhale ndi cikwati cacimwemwe ndi copambana . ( Chivumbulutso 21 : 4 , 5 ) Mapeto a dziko si mapeto a moyo wanu ai . Vicky anaona kuti cinthu cofunika kwambili ndi kuika Yehova ndi mfundo zake patsogolo osati zinthu zakuthupi . Ndipo ngati sindinaphunzitse ena , mpingo sungalephele kuyenda bwino . ’ N’zocititsa cidwi kuti Paulo anayamba kufotokoza ulosi wa masiku otsiliza ndi mau akuti “ dziŵa kuti . ” 1 : 5 , 18 ; Akol . Kumbukilani mmene Paulo anavutikila na cikumbumtima na kupwetekedwa mtima cifukwa cokhala mu ukapolo wa ucimo na imfa . Iye atabatizidwa , tinakhala m’nyumba imodzi kwa kanthawi ndithu . Mungapewe zinthu zimene zingabweletse nkhawa zosiyana - siyana . Mudzapindulanso mwa kupewa zinthu monga “ kuwawidwa mtima konse kwa njilu , kupsa mtima , mkwiyo , kulalata ndiponso mau acipongwe . ” — Aef . N’nali kufuna kuti anthu akuda akhale na ufulu woculuka , cifukwa pa nthawiyo tinali kucitilidwa zinthu zambili zopanda cilungamo . Zoipa za tsiku lililonse n’zokwanila pa tsikulo . ’ 11 : 49 - 53 ; 18 : 14 Kuti timvetsetse mfundo imeneyi , tiyelekezele motele : Tinene kuti tate anashanga maluŵa ambili okongola pa nyumba . Mofanana ndi Paulo , mwina inunso mwalimbikitsidwapo ndi abale ndi alongo a mumpingo wanu . Tingawathandize pa zinthu zing’ono - zing’ono monga kuwadziŵitsa za mayendedwe , kumene angagule zakudya zopatsa thanzi koma zochipa , ndiponso mmene angapezele zipangizo zogwilila nchito monga mashini osokela kapena okhwapila udzu , kuti azipezako ndalama . Gavin anadalitsidwa cifukwa cophunzila Baibulo ndipo anapeza mayankho a mafunso ake onse . Pamene izi zinali kucitika , Katharina anali atacoka kale m’delalo . Ngakhale kuti si ca m’Malemba ndipo sicoyenela kuti akulu azipanga malamulo okhudza kagwilitsidwe nchito ka pelefyumu pobwela ku misonkhano , io angadziŵitse mpingo za mavuto amene ena akukumana nao cifukwa ca pelefyumu . ( Ŵelengani Yohane 15 : 9 . ) Koma n’cifukwa ciani Mulungu amalola zimenezi kucitika ? Kodi amuna ambili a m’gawo lanu amavutika kuti apeze zinthu zofunika paumoyo ? ( b ) Kodi iye akanakhala ndi maganizo olakwika ati ? Mwa kulalikila uthenga wa Ufumu . Nthawi iliyonse pamene tilengeza uthenga wa Ufumu , timakhala ngati tikufesa mbewu zolingana ndi zimene zinafesedwa mumtima mwathu . Ŵelengani na colinga cakuti muimvetsetse . Iye anali kukhulupilila zonse zimene Yesu anali kuphunzitsa , ndipo sanakaikile kuti anali Mesiya wolonjezedwa . Ngalawa imene Paulo anakwela kupita ku Italiya inali kulimbana ndi mafunde panyanja . Katherine anapempha Yehova kuti am’thandize kupeza mlongo woyenelela amene angaziwaphunzitsa . N’ciani cimene Nowa anapitiliza kuyembekezela pambuyo pa Cigumula ? Mayankho a mafunso awa angatithandize kuyandikila kwambili Yehova ndi kumulambila ndi mtima wathu wonse . ( Salimo 2 : 4 - 8 ) Yesu adzapulumutsa anthu osauka ndipo adzathetsa kupondelezana komanso ciwawa . — Ŵelengani Salimo 72 : 8 , 12 - 14 . Onani zitsanzo ziŵili zotsatilizi . Mpaka tsiku lina ndinafikila aphunzitsi kuti ndiwafotozele za cikhulupililo canga . Tiyeni tikambilane zinthu zina zimene mungacite . NYIMBO : 54 , 125 Pambuyo pakuti msilikali wandiyesa kuti aone ngati ndingakwanitse , anandiuza kuti , “ Iwe wapambana onse m’gulu lako . ” Ndi dipo lotani limene linakwanilitsa cilungamo ? Abale ndi alongo ambili anakhalabe okhulupilika pamene anali kuyesedwa kuti atengeko mbali m’ndale . ( a ) Kodi Akristu amapindula bwanji akamaganizila za ciyembekezo cao ? ( Aheberi 10 : 24 ) Koma zimenezi sizitanthauza kuti tiyenela kulowelela nkhani za ena . Koma kodi tingaphunzitse bwanji cikumbumtima cathu ? Riana anati : “ N’nali kukamba nkhani ya anthu onse pakangopita wiki imodzi . Kodi anali kuganizila za kucepa kwa copeleka cake poyelekezela ndi zimene akanapeleka mwamuna wake akanakhala ndi moyo ? Mwacitsanzo , ku Spain , mamiliyoni a anthu acikatalani , amakamba cinenelo cao ca Cikatalani nthawi zonse . Iye anati : “ Aliyense woyang’anitsitsa mkazi mpaka kumulakalaka , wacita naye kale cigololo mumtima mwake . ” ( Mat . Tsiku lililonse , timafunika kusankha pankhani ya zosangulutsa , kavalidwe na kudzikongeletsa , mmene tingaseŵenzetsele ndalama , ndi mmene tingakhalile ndi ena . Ngati io alandila uthenga wabwino ndi mtima wonse , adzalandila madalitso mtsogolo . Iye anali mwana wacitsanzo cabwino , koma mwadzidzidzi anayamba kucita zinthu zoipa . Conco , io sadzafa cifukwa ca uchimo . 14 : 21 , 22 ) Mau amenewa ukangowamva samveka olimbikitsa . 43 : 10 - 12 . ( b ) Tiphunzilapo ciani za Yehova tikaganizila mmene iye anacitila zinthu na Yobu ? 3 : 5 , 6 ; Afil . ( Sal . 32 : 1 - 5 ) Mofananamo , masiku ano mtumiki wa Yehova amacotsedwa mumpingo pokhapo ngati ndi wosalapa kapena akupitilizabe kucita chimo . Cimeneci cinali cipambano cacikulu . Tikakumana ndi vuto ladzidzidzi , tingapemphe thandizo kwa Yehova ndipo iye amasangalala kumva mapemphelo otelo a anthu olungama . ( Sal . 34 : 15 ; Miy . ( b ) Ni malangizo ena ati amene apezeka m’Mau a Mulungu ? Nanga n’cifukwa ciani tiyenela kuwatsatila ? Yehova , Mlembi wa Baibulo , afuna kuti anthu adziŵe dzina lake . Nkhondo itangoyamba , anthu anafunsa mtsogoleli wa dziko la Germany kuti , “ Kodi n’ciani cayambitsa nkhondo ? ” Kodi tingati kumeneko n’kudzicepetsa ? N’cifukwa ciani kuyeletsa ndi kukonza zoonongeka pa Nyumba ya Ufumu nthawi zonse n’kofunika ? Anthu pafupi - fupi 70 miliyoni anafa ndi njala kuyambila m’caka ca 1901 mpaka mu 2000 . Koma mukudziŵanso kuti kukhala wokhulupilika kwa Yehova ndiye kofunika kwambili . Sitingazimvetsetse . ” Iwo adzakamba kuti : “ Iye akatiphunzitsa njila zake , ndipo ife tidzayenda m’njila zakezo . ” Komanso , tidzalola mphamvu ya Mau a Mulungu kugwila nchito mokwanila mu umoyo wathu . — 2 Akor . Kodi Mumayendela Limodzi ndi Gulu la Yehova ? 5 / 1 Koma cinacake cinanipangitsa kutumila foni mayi wa panyumbapo . ” ( Ŵelengani Miyambo 15 : 28 . ) Maphunzilo apamwamba amenewo anacititsa Mose kukhala “ wamphamvu m’mau ndi m’zocita zake . ” Nchito yathu ya padziko lonse yophunzitsa anthu Baibo ndi kuthandiza anthu okhudzidwa ndi mavuto aakulu , imacilikizidwa na ndalama zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo . Kutatsala mwezi umodzi kuti tikondwelele zaka 40 za cikwati cathu , mkazi wanga Eunice anamwalila na matenda a khansa . Mabwana ambili sayamikila anchito awo . Iwo anapita kukafuna nchito ku makampani okonza za magetsi ndi a migodi ndipo anakhala ku midzi ya ku Victoria . Wolemba buku limeneli anakamba za iwo ndi ena kuti “ anacitilidwa umboni cifukwa ca cikhulupililo cawo . ” M’kupita kwa nthawi , akuganizilanso zimene angacite kuti ayenelele kukhala woyang’anila . Muziika zofuna za ena patsogolo pa zofuna zanu . Pelekani citsanzo coonetsa kuti Yehova amadalitsa anthu amene amafuna kuyeletsa dzina lake . Amuna acikristu safunika kukakamiza akazi ao kuti aziwalemekeza . Ngati ndinu mmodzi wa acinyamatawo , kodi simuona kuti ndi mwai wamtengo wapatali kudziŵa Mlengi ndi kumtumikila ? Tinali kucita izi pofuna kupewa maceza amtatakuya , amene akanacititsa kuti tiyambe kukangana pa nkhani za cipembedzo . ” Gwilitsilani Nchito Mau a Mulungu Ndi Amoyo Ndipo Yehova anacita zozizwitsa zambili kuti akwanilitse lonjezo limenelo . Kodi colinga ca Yehova cokhudza anthu omvela cimaonekela bwanji m’pemphelo la citsanzo ? Ngati zimenezi ndi zimene ana anu amacita kodi mungacitenji ? Ni wosokoneza cikondi , mtendele , na mgwilizano m’mipingo . Palibe Mkhiristu wokhulupilika amene angafune kukhala wopanda ulemu kapena wosakhulupilika monga Diotirefe . Cifukwa n’ciani timanena kuti si anthu onse a m’zipembedzo amene adzaphedwa pamene Babulo Wamkulu adzaonongedwa ? Ponena za munthu wokhulupilika Yobu , Mdyelekezi anauza Mulungu kuti : “ Kodi inuyo simwam’chinga iyeyo ? Anthu a Yehova amakumana kuti alambile Mulungu mu Nyumba za Ufumu ndi malo ena masauzande ambilimbili padziko lonse lapansi . N’cifukwa ciani Yehova anayesa kum’thandiza Kaini ? Tonse timafunikila ndalama . “ Zinthu izi mwazibisa kwa anzelu ndi ozama m’maphunzilo , koma mwaziulula kwa tiana . ” — LUKA 10 : 21 . A Yohane : Inde . Zipatso zambili zimapsa bwino pamene dzuŵa likuwala bwino . Ndikakumana ndi mavuto ndimapemphela . Popeza lomba tili na cisomo ca Mulungu ndipo timakhululukidwa macimo , kodi ndimwe ofunitsitsa kupewa ‘ kupelekanso ziwalo zanu ku ucimo ’ ? ( Ŵelengani Miyambo 20 : 5 . ) 31 KODI MUDZIŴA ? Kabokosi kali pa tsamba 16 kasonyeza zifukwa zina . Dziŵani kuti pali zinthu zambili zimene simungakwanitse kucita , ndipo mukalakwitsa muzivomeleza . 3 : 9 ) Conco , tiyeni tiziyesetsa tsiku lililonse kuonetsana cikondi , cimene ndi khalidwe lamtengo wapatali limene mzimu woyela wa Mulungu umabala . Ulosiwu udzakwanilitsidwa kupitila mwa Yesu , Mfumu yodzozedwa na Mulungu . ( Mac . 15 : 1 , 2 ) Motsogoleledwa na mzimu komanso pambuyo pokambilana mfundo za m’Malemba , abale a m’bungwelo anaona kuti kucita mdulidwe sikunali kofunika . Mwa ici , analembela kalata mipingo yofotokoza cigamulo cawo pa nkhaniyi . ( b ) N’ciani mwina cimene cinapangitsa Asa kudalila anthu pamene Basa anaukila dziko la Yuda ? Mbali yoyamba , zioneka kuti Asaduki pom’funsa anali kuganiza za ciukililo ca padziko lapansi , ndi kuti Yesu anawayankha moyenelela . ( Gen . 41 : 37 - 44 ; 45 : 4 - 8 ) Ngati mukumana ndi mavuto , muzipemphela kuti Mulungu akupatseni nzelu , muzikamba ndi kucita zinthu modekha , ndipo muzidalila Mulungu kuti akulimbitseni . Makolo anga anacita cidwi na khalidwe la mpainiya wacicepele wodzipeleka ameneyu , cakuti anam’pempha kuti azikhala nawo . Nchito imeneyi imatipatsa cimwemwe , imatiteteza komanso imalimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova ndiponso anzathu ( Chiv . 14 : 6 ) Mwacitsanzo , pamene tinali kukonza zakuti Nsanja ya Mlonda izimasulilidwa m’Citongani , ndinakumana ndi akulu onse olankhula Citongani . Kuti tipeze yankho , tiyeni tikambilane mbili ya m’Malemba ya alambili oona a Yehova . 18 : 37 . Kodi n’cifukwa ciani Ayuda analeka mwamsanga conco kugwila nchito imene Mulungu anawapatsa ? Panthawiyo , kapolo wokhulupilika anali kukamba kwambili ndi anthu a Mulungu m’Cingelezi . Mboni za Yehova zonse ziyenela kupatsidwa cakudya kaŵili pa tsiku , popeza kuti io sanalakwe koma ali kuno cifukwa ca zikhulupililo zao zocokela m’Baibulo . ” Komabe , anthu ena amaona kuti zocita zao zimacititsa kuti Mulungu asaziwaŵelengela . M’bale Peter , amene ali ndi zaka 75 anati : “ Muziona zinthu moyenela . Nchito yolalikila ya padziko lonse ya Mboni za Yehova yathandiza anthu kuzindikila ciani ? Yehova * adzapitiliza kutithandiza ngati tikupitiliza kucita cifunilo cake . Mwina tinali na mwayi wocita maphunzilo apamwamba , wokwezedwa pa nchito , kapena wopeza ndalama zambili pocita bizinesi inayake . Kodi anthu anaonetsa bwanji tsankho kwa ophunzila a Yesu ? Anamwali onse 10 anafunika kukhala maso , ndipo nyali zao zinafunika kupitiliza kukhala zoyaka usiku . KWA ACICEPELE Ambili mwa iwo ni acicepele amene makolo awo ni Mboni . Acicepele amenewa anasankha umoyo wabwino kwambili . ( Sal . Mabanja ambili amaŵelengela pamodzi cigawo ca m’Baibulo . Masiku ano , ndimaona kuti ndikanalemekeza maganizo a amai ndi zikhulupililo zao pokamba nao , zinthu zikanayenda bwino . Kodi zinangocitika mwangozi kuti Kenneth atume foni panthawi yoyenela ? Conco , anthu a Yehova padziko lonse lapansi amavala mogwilizana ndi kumene amakhala kuti asakhumudwitse ena . Masiku ano , anthu amakonda kutumilana mauthenga pafoni kapena pa Intaneti . OPHUNZILA a Yesu 7 anacezela usiku wonse pa Nyanja ya Galileya kuti aphe nsomba , koma sanaphe kanthu . Pamisonkhano yathu , timapemphela kwa Yehova , kumuimbila , ndi kupeleka ndemanga . Zimenezi zimam’kondweletsa Padziko lonse pali ansembe a Cikatolika okwana 400,000 , koma pali Mboni za Yehova zoposa 8 miliyoni zimene zikulalikila uthenga wabwino m’maiko 240 . Anakambanso kuti : ‘ Yehovayo ndiye watiuza kuti tiwononge dziko lanu . ’ Kodi N’zoona Kuti Anthu Anali Kubyala Namsongole m’Munda ? Mwacitsanzo , tate wina ku Mexico amacoka panyumba 6 koloko mmaŵa , ndipo amabwelela kunyumba 8 koloko usiku . Ena amene anamanga banja posacedwapa amapempha malangizo a zimene angacite kuti banja lawo liyende bwino . ( b ) N’ciani cionetsa kuti Amosi anali munthu wodziŵa zinthu ? Apainiya amene analibe makalavani anali kugwilitsila nchito njinga kukalalikila m’madela akutali . Ku Roma wakale , Akristu anali ndi maganizo osiyanasiyana pankhani ya zakudya zina ndi mapwando . * Komabe , m’Baibo imeneyi , dzina la Mulungu limapezeka m’malo ocepa kwambili . Caka ciliconse , anthu amathela nthawi yaitali kusakila mphatso yabwino “ koposa ” imene angapatse mnzawo , kapena wacibululu wawo pa cocitika capadela . ( a ) Kodi cikondi n’ciani ? Mwacitsanzo , kodi muli ndi cofooka cinacake cimene mukulimbana naco ? Zimenezi zionetsa kuti Yehova ndi wanzelu kwambili . Mofanana ndi zofufumitsa za m’fanizo la Yesu , uthenga wa Ufumu unakula ndi kusintha miyoyo ya anthu ambili , ndipo Franz ndi Margit akusangalala kwambili . Naonso ofalitsa ena amene angathe kucita upainiya , amazengeleza kuyamba utumiki umenewo . Davide sanafune kuti anthu adziŵe zimene anacitazo . 2 : 3 , 4 ) Mkati mwa nthawi imeneyi , Mfumu yosakhulupilika Sauli inali kusaka - saka Davide kuti imuphe . Yehova anamuona kuti anali mlimi wocenjela ndi wanzelu , ndipo anam’gwilitsila nchito . Iwo amafunikila kukhala okhulupilika ku dziko lao . ( Luka 11 : 9 , 13 ) Pamene mupempha mzimu woyela , muzipemphanso cikhulupililo coonjezeleka . Ofalitsa a Ufumu ambili amakonda ulaliki wapoyela ndi kuuza anthu za webusaiti yathu ( Onani ndime 12 ndi 13 ) Njilayi ndi kompyuta imene poigwilitsila nchito amaseŵenzetsa maso ake . ( Aheberi 2 : 1 ; 3 : 12 ) Yesu anaticenjeza kuti ngati sitimvela kapena kulandila Mau a Mulungu ndi “ mtima woona komanso wabwino , ” ‘ sitingawagwilitsitse . ’ Koma ngati makolo sangakhale okha pangafunikile kupeza njila ina yoŵasamalila . Kodi munagulapo zinthu zimene simunali kufunikila cabe cifukwa cakuti zinali kuoneka zokongola kapena cifukwa cokopeka ndi zokamba za otsatsa malonda ? Apa n’kuti afilisiti akukonzekela kuwathila nkhondo , ndipo Aisiraeli ena anali atayamba kucoka kwa Sauli . ATUMIKI a Yehova amalemekeza kwambili buku lake loyela , Baibo . Conco , okwatilana ayenela kulimbitsa cikwati cao mwa kulankhulana mokoma mtima , mwacikondi , ndi mwacifundo . — Aef . Zimenezi zinacititsa kuti Koresi aononge mzindawo mosavuta . Pamene anali na zaka 18 , wapolisi wina anayamba kumunyengelela kuti acite naye ciwelewele , koma iye anakanitsitsa . Ndi zinthu zotani zimene tingasinkhesinkhe ? 15 , 16 . ( a ) Ndi ziyeso zina ziti zimene tifunika kupewa ? Koma Farao sanalole Aisiraeli kuti apite . Kuti Yehova apulumutse anthu ake , anabweletsa milili 10 pa Iguputo . Pambuyo pake , anaononga Farao ndi gulu lake la nkhondo pa Nyanja Yofiila . ( Eks . Mawu a Yehova amenewa ndi olimbikitsa kwambili . Iwo akhoza kudziona osayenelela kukhala pakati pa mitundu ina cifukwa ca mmene analeledwela kapena cifukwa ca mmene zinthu zilli paumoyo wawo . 8 : 6 , 7 ) Kunena zoona , anthu amene amakonda kufuna - funa zinthu zakuthupi kapena kukhutilitsa cilakolako cawo ca kugonana , amagwilitsidwa mwala , ndipo amadzibweletsela mavuto ambili . — 1 Akor . ( Yesaya 46 : 10 ) Inuyo ndi banja lanu mungakhale ndi tsogolo labwino . Kenako analangiza Akristuwo kuti : “ M’cotseni pakati panu munthu woipayo . ” — 1 Akor . ( b ) Nanga anadalitsidwa bwanji cifukwa ca kulimba mtima na kukhulupilika kwake kwa Mulungu ? Dipo inacititsa kuti pakhale ciyembekezo ca kuuka kwa akufa . Caciŵili , tili na umboni wotsimikizilika wa anthu amene Mulungu anawatonthoza , a m’nthawi yathu ndi a m’nthawi yakale . Atazindikila kuti ngaleyo ndi yamtengo wapatali , wamalonda uja “ mwamsanga ” anali wofunitsitsa kugulitsa zinthu zonse zimene anali nazo kuti akagule ngaleyo . Muzitsimikizila nkhaniyo mutamva umboni wa pakamwa pa mboni ziŵili kapena zitatu . ” ( Yuda 17 , 18 ) N’ciani cingatithandize kuti tikhale ‘ otsimikiza mtima kwambili ’ kukana kudya kapena kuikidwa magazi ? — Deut . Ndithudi , zimene Paulo anacenjeza zokhudza zotulukapo zake ngati munthu ‘ aika maganizo pa zinthu za thupi , ’ ziyenela kulimbikitsa Akhiristu kupanga masinthidwe ofunikila . Kenako anakamba kuti : “ Koma n’nali kuona monga siningakwanitse kukatumikila kosoŵa . ” ( Yesaya 48 : 17 ) M’nkhani ino , tikambilana mfundo zitatu zimene zingatithandize kuti tizipindula ndi cakudya cakuuzimu cimene Yehova amatipatsa . Ngati mwakwanitsa kukhazikitsa mtendele ndiye kuti ‘ mwabweza m’bale wanuyo . ’ ( Luka 21 : 20 , 21 ) M’masiku ano otsiliza pali gulu latsopano limene limaimila Yehova . Anthu ambili amene amapita ku maiko ena anakulila m’mabanja mmene amalemekeza kwambili miyambo ndi makolo . ( Gen . 3 : 8 ) Koma pokhala woweluza wolungama iye coyamba anamvetsela kwa Adamu ndi Hava . ( Gen . ZIMENE ANAPHUNZITSA : Mmodzi wa ophunzila a Yesu anamupempha kuti , “ Ambuye tiphunzitseni kupemphela . ” Ndiyeno Yesu anayankha kuti : “ Mukamapemphela muzinena kuti ‘ Atate . ’ ” Iye anali kunimvetsela moleza mtima nikamamuuza mavuto anga . NYIMBO : 18 , 14 Sindingacite zimenezi pamaso pa Yehova . Sindingatambasule dzanja langa ndi kukantha wodzozedwa wa Yehova . ” — 1 Samueli 26 : 8 - 12 . Koma anthu ena ali muno cifukwa cakuti anapha anthu . Lolani Yehova kuti azikamba nanu masiku onse kudzela m’Mau ake . Nthawi ina ndi pamene anali kuthaŵa Sauli . Iye anali wanzelu , koma mwamuna wake Nabala anali woipa mtima , wacabecabe , ndi wopanda nzelu . ( 1 Sam . M’bale wina wa ku Sri Lanka , amene lomba akhala ku dziko lina , anapeleka malo ndi nyumba yake m’dziko lawo kuti abale azicitilapo misonkhano yampingo ndi yadela , komanso kuti pazikhala atumiki anthawi zonse . Nayenso munthu amene waleka kusambila atatsala pang’ono kufika kumtunda , amamila . John anapitiliza kuti , “ Izi zinapangitsa kuti mkazi wanga azisamalila mwana wathu komanso ineyo ndiponso kundipelekeza kukaonana ndi dokotala . ” Iwo sanalakwile cabe akulu - akulu a Boma ndi gulu lankhondo la asilikali , komanso anyozela azibusa onse a machechi . KODI MAVUTO AMACITIKA CIFUKWA CA KARMA ? Ngati mungafunse Mhindu kapena Mbuda funso limene lili pacikuto ca magazini ino , adzakuyankhani kuti : “ Zinthu zoipa zimacitikila anthu abwino cifukwa ca lamulo la Karma . Zinanitengela Nthawi Yaitali Kuti Nisinthe 12 M’baleyu ananipatsa njinga yakale yoti niziyendelapo polalikila m’gawo langa , limene kunali mapili ambili . Kuyambila pamenepo , amayi anakhala na cidwi cofuna kudziwa coonadi . Pambuyo pakuti Tatenai wabwelako ku Yerusalemu kumene anakafufuza za mlandu wa Ayuda , iye anapeleka lipoti kwa Dariyo kuti Ayuda anakamba kuti Koresi ndiye anawalamula kumanganso kacisi wa Yehova . ATUMIKI A MULUNGU ANAPULUMUKA N’ciani cinacitikila Yerusalemu wakale ? ( Danieli 12 : 4 ; Aroma 11 : 33 ) Baibulo limatiuza zambili zokhudza Mulungu “ amene anapanga kumwamba ndi dziko lapansi . ” Yelekezelani kuti mufunika kuteteza zimene mumakhulupilila pamaso pa mfumu yotelo . Mwacitsanzo , acicepele ambili amadzipeleka kugwila nchito yomanga . TSAMBA 28 • NYIMBO : 95 , 100 Iye amacita cifunilo ca Yehova osati cake , ndipo amatsatila Yesu mosamala kwambili mu zocita ndiponso zokamba zake . Kodi cimatanthauza cabe kuvomeleza kuti Mulungu adzatipatsadi zimene walonjeza ? Ndipo timacita zimenezi mwa kulalikila mwakhama uthenga wabwino ndi kupanga ophunzila . Kumisonkhano , ndinapeza abale ndi alongo ambili amene anali kutsutsidwa ndi acibale ao . ( Yes . 5 : 20 ) Yesu anacenjeza ophunzila ake kuti : “ Nthawi ikubwela pamene aliyense wakupha inu adzaganiza kuti wacita utumiki wopatulika kwa Mulungu . ” ( Yoh . Ndiyeno ganizilani mfundo zimene Baibo imaphunzitsa . Nanga bwanji za madalitso amene tiyembekezela mtsogolo ? Yesu anali kukonda kuuza anthu za Ufumu wa Mulungu . Yesu anati : “ Musadabwe nazo zimenezi , cifukwa idzafika nthawi pamene onse ali m’manda acikumbutso adzamva mau [ anga ] ndipo adzatuluka . ” ( Yoh . Ndinasangalala Ndi Mayankho Omveka Bwino a m’Baibulo 10 Mungagwilitsile nchito kabuku kacingelezi kakuti The Origin of Life — Five Questions Worth Asking , kuti mupeleke mayankho omveka kwa anthu ofuna kudziŵa za “ ciyembekezo cimene muli naco . ” ( 1 Pet . Pa msonkhano wadela ku India mu 1948 18 Kodi Tingalimbitse Bwanji Mgwilizano Pakati Pathu ? 21 : 10 , 11 ) Buku la Chivumbulutso limafotokoza za ulemelelo wa Yerusalemu Watsopano mocititsa cidwi . 5 : 5 ) Izi n’zosadabwitsa cifukwa kudzipeleka na kubatizika ni nkhani yaikulu , komanso ni mbali yofunika kwambili mu umoyo wa Mkhristu . — Onani bokosi yakuti “ Kodi Munadzipeleka kwa Yehova ? ” Mukamafotokoza zinthu mwacindunji m’pemphelo , zimakhala zosavuta kudziŵa kuti Yehova wayankha pemphelo lanu . Ngati mumasankha nyimbo , mabuku , ndi mafilimu oyenelela , mumaphunzitsa ana anu kucita cimodzimodzi . — Aroma 2 : 21 - 24 . Wokwelapo akucititsa anthu ambili kufa cifukwa ca matenda na zinthu zina . Muzikhala na zocita zambili potumikila Yehova . ( Sal . Kodi Yehova adzathetsa bwanji makhalidwe oipa ? 19 : 12 - 22 ) Loti anamvela ndipo ana ake aakazi naonso anathawa mumzindawo pamodzi ndi iye . Alendowo anali kuyenda cifukwa ca uthenga wabwino . Cifukwa ca mavuto a zacuma , nthawi zambili mabanja amasamukila kudziko lina kuti akapezeko thandizo . Motelo kucokela nthawiyo , m’Yelusalemu munalibe mfumu imene inali kuimila Yehova . Kuŵelengela nthawi kwa m’Baibulo ndi zocitika za padzikoli zimasonyeza kuti nkhondo ya kumwamba imeneyi inacitika pambuyo pakuti Ufumu wa Mulungu wakhazikitsidwa kumwamba mu 1914 . 51 : 4 , 6 , 10 , 11 . POKHALA Mboni za Yehova , timalalikila kuti Ufumu wa Mulungu ndiwo wokha umene udzathetsa mavuto athu onse . Mofunitsitsa timauzako anthu coonadi cimeneci ca m’Malemba . CAKA catha , abale masauzande ambili anaikidwa kukhala akulu na atumiki othandiza m’mipingo ya Mboni za Yehova pa dziko lonse lapansi . [ Mau apansi ] Onani caputala 8 m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni . lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . [ Bokosi papeji 6 , 7 ] Kodi n’ciani cingatithandize kuti tizipezeka pamisonkhano nthawi zonse ? Kodi Yesu anafunikila kuyamba liti kulamulila monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu ? Komabe , Paulo anakamba kuti abalewo anayamba ‘ kubwelelanso ’ ku zinthu zopanda pake . Kamvedwe katsopano : Yesu akadzabwela mtsogolo , adzafupa akapolo ake odzozedwa okhulupilika mwa kuwapatsa mphoto yao ya kumwamba . Mosakayikila . Poganizila citsanzo cimeneci , mungacite ciani ngati muona kuti mwana wanu amamvetsetsa ziphunzitso zoyambilila za m’Malemba , kuphatikizapo tanthauzo ndi kufunika kodzipeleka na kubatizika ? ( 1 Samueli 17 : 23 , 26 , 48 - 51 ) Ndipo Davide atakhala mfumu , mneneli wa Yehova Natani anam’patsa uphungu cifukwa ca macimo amene anacita . 25 : 1 - 5 , 9 . Panopa mu Zambia muli ofalitsa oposa 170,000 , ndipo anthu oposa 763,915 anapezeka pa Cikumbutso mu 2013 . Kodi timapatsa moni alendo akabwela pa Nyumba ya Ufumu ? 3 : 16 , 17 ) Conco , muzifufuza mfundo za m’Malemba n’colinga cakuti muthe “ kuzindikila cifunilo ca Yehova . ” 7 : 2 , 3 ) Pamene Abulahamu anali ku Harana , paulendo wake wopita ku Kanani , Yehova anamuuza kuti : “ Tuluka m’dziko lako , pakati pa abale ako , ndi kusiya nyumba ya bambo ako . Upite kudziko limene ndidzakusonyeza . Yehova akupeleka malangizo othandiza kwa munthu aliyense ( Onani ndime 16 ndi 17 ) Ena angamayambe n’kupanga cosankha , ndiyeno n’kupemphela kuti Yehova adalitse cosankha cawo . Yehova amatipatsa malangizo pofuna kutiteteza ku mavuto ngati amenewa . — Ŵelengani Yesaya 48 : 17 , 18 . Poimba , muzikwezako m’mwamba buku lanu la nyimbo , kuwelamutsa mutu , na kuimba mocokela pansi pa mtima . Mlongo wina wa ku Albania analembanso kuti : “ Mau a Mulungu akumveka bwino kwambili m’Ciabaniya ! Taona kuti zina zimene tifunika kucita kuti tikonze cipulumutso cathu ni kuŵelenga Mau a Mulungu na kuwasinkha - sinkha , kupemphela kwa Yehova , na kuganizila mmene iye watidalitsila mu umoyo wathu . 27 Muzicilikiza Ulamulilo wa Yehova Conco okana Kristu aphimba coonadi conena za Yehova Mulungu ndi Yesu Kristu . Ngakhale kuti Yesu sanafotokoze cifukwa cake anakamba kuti cuma ni “ cosalungama , ” Baibo imaonetselatu kuti kucita malonda si mbali ya colinga ca Mulungu . ( Aefeso 5 : 26 ) Ngati anthu ankhanza ndi odzikonda aphunzila Baibulo , angasinthe n’kukhala okoma mtima ndi amtendele . Ndiyeno analangiza kuti : “ Cofunika ni pemphelo kuti ukhalebe wokangalika potumikila Yehova . Koma pali anthu ena mumpingo amene angaone ngati alibe luso lililonse . Amenewa angaphatikizepo Akristu obatizika , acicepele , ndi acatsopano . M’bale Ray Bopp wa ku mpingo wa Chicago anakamba kuti m’zaka za m’ma 1910 , kuyendetsa zizindikilo pa cikumbutso kunali kutenga maola ambili cifukwa pafupifupi anthu onse ofika pa mwambowo anali kudya zizindikilozo . Yehova amatithandiza notiphunzitsa kuti tipambane . 34 : 6 . 7 : 9 , 10 , 14 . Zaka mahandiledi angapo Estinne asanababwe , akatswili olemba mabuku aciyuda , anali atagaŵa kale Baibulo la Ciheberi kapena kuti Cipangano Cakale kukhala m’mavesi koma osati m’macaputala . “ Baibulo ndi buku la cipembedzo lodziŵika kwambili . N’cifukwa ciani Yehova amatikhululukila ? Nanga tifunika kumva bwanji ndi zimenezi ? Komabe , nchito yaikulu imene Akristu akupemphedwa kucita ndi nchito yolalikila . ( b ) Kodi “ dzanja ” la Mulungu limatanthauza ciani ? Baibulo limati , ‘ nthawi yatsoka ndi zinthu zosayembekezeleka zimatigwela tonsefe . ’ Conco , monga ‘ otsanzila Mulungu , ’ tiyeni ticite zonse zimene tingathe kuti tizilandila alendo amene ali pakati pathu . — Aef . Ngati tipempha mwa njila imeneyi , Mulungu “ amatimvela . ” Iwo ni ogwilizana ndiponso osangalala cifukwa ca zimene Yehova amawaphunzitsa . Nkhaniyi idzafotokoza mmene acinyamata ndi acikulile angathandizilane pa kusintha kumeneku . 11 : 30 - 35 . Yesu anafotokoza cifukwa cake anthu ena adzalandila moyo wosatha pamene ena adzaonongedwa . M’malo mwake , anatsimikiza mtima kukonda Yehova ndi mtima wake wonse , moyo wake wonse ndi mphamvu zake zonse . ( Deut . ( b ) Tidzakambilana funso lakuti ciani m’nkhani yotsatila ? Pofuna kuonetsa kuti angelo ali ndi cinenelo ndipo amalankhula , Baibo imakamba za “ malilime a anthu ndi a angelo . ” Kodi n’ciani canithandiza kukhalabe wolimba mwauzimu zaka zonsezi zimene nakhala mumpingo wa Cizungu , kucokela mu 1946 ? Onse anayi akutumikila monga akulu . Ndimadziŵa kuti Baibulo ndi buku labwino , koma sindinali kudziŵa kuti ndi buku la mbili yakale . 6 : 4 , 6 ; 1 Tim . ZIMENE BAIBULO LIMAKAMBA Kodi Mose anapindula bwanji cifukwa coganizila zimene Mulungu analonjeza ? Amene amacita utumiki wanthawi zonse amapeza madalitso ambili ( Onani palagilafu 11 - 13 ) Pa cifukwa cimeneco , dziko lapansi lidzasungidwa monga colengedwa ca Mulungu ndipo iye adzalisunga kosatha . ” Ndinali ndi mtima wapacala . Kukula mwakuthupi monga kutalika kapena kuina , kumaonekela mosavuta kwa ena . Koma n’kosiyana na kukhwima m’maganizo cifukwa kumatenga nthawi yaitali kuti kuonekele kwa ena . Pambuyo pake , panabukanso nkhondo yaciŵili ya dziko lonse imene inawononga koposa . Yosimbidwa ndi David ndi Gwen Cartwright Kodi mungalemekeze bwana wanu amene amavomeleza akalakwitsa kapena amene sapepesa ngakhale pang’ono ? “ Kuti tipitilize kukhala na moyo komanso maganizo abwino , tifunika kudziŵa colinga ca moyo . ” Analemba conco pulofesa wina wa zamaganizo a anthu dzina lake , William McDougall . Koma ndife otsimikiza kuti Atate wathu wakumwamba amaona khalidwe lathu la kuona mtima ndi makhalidwe ena abwino kukhala amtengo wapatali kuposa zinthu zakuthupi zilizonse . Kuwonjezela apo , adzafunika kumvela malangizo atsopano olembedwa “ m’mipukutu , ” ofotokoza mmene Yehova afuna kuti iwo adzikhalila m’dziko latsopano . Zaka 300 m’mbuyomo , Yehova anali atalamula Aisiraeli kupha anthu onse olambila mafano m’Dziko Lolonjezedwa , koma io sanamvele . ▪ Boma lakumwamba la Mulungu ndi limene lidzaononga anthu onse oipa ndi osamvela osati maboma a anthu padziko . Ngati tiyesetsa kukhululukilana masiku ano ndi kukhala paubwenzi wabwino ndi ena , sicidzakhala covuta kucita zimenezi panthawiyo . — Ŵelengani Akolose 3 : 12 - 14 . Kodi Mudzatengelapo Phunzilo pa Zimene Zinalembedwa ? Kuonjezela pa kutumikila Yehova , kodi n’zosankha zofunika zina ziti zimene zingakhudze utumiki wanu kwa Mulungu ? Zimene Paulo anakamba zinawacititsa cidwi cakuti anafuna kumva zambili . Popatulila kacisi , kuimba nyimbo kunali mbali yofunika kwambili . Komanso panali masaka a magazini amene anali kufunika kupelekedwa ku positi ofesi n’colinga cakuti awatumize ku mipingo yonse ya m’dziko la United States . N’cifukwa ciani Akristu oona sayenela kupeputsa malamulo a Mulungu ? Ngakhale kuti abalewa alibe mwayi wosamalila makolo awo okalamba kapena wokwatila , ndipo amazunzidwa kwambili , sanagwedezeke pa cikhulupililo cawo . Caciŵili , kumbukilani nthawi imene munapita ku msonkhano wacikristu . “ Asayansi ambili amaganiza kuti . . . anthu ndi amene ayenela kuimbidwa mlandu woononga mitundu yosiyanasiyana ya zacilengedwe , ndipo zimenezi zikucitika mofulumila kwambili masiku ano . ” — From science.nationalgeographic.com . Ndingacite ciani kuti ndizicita zimene Baibulo limakamba ndi kupitiliza kusintha umunthu wanga ? ’ Zimenezi zinathandiza kuti anthu amene anali kuphika ndi kupelekela cakudya azimvetsela mapulogilamu ndi kusangalala ndi maceza olimbikitsa . N’cifukwa cake imfa ilibe kuti n’nazoloŵela . N’ndani amene safuna kukhala na cikhulupililo ca conco ? Vuto la Ziphuphu za m’Boma 3 ( Yohane 13 : 34 , 35 ) M’zaka za posacedwapa , atumiki a Yehova aonetsa kuti amakondana ngakhale pa nthawi ya nkhondo . CITANI ZINTHU MWANZELU : “ Akazi azidzikongoletsa ndi zovala zoyenela , povala mwaulemu ndi mwanzelu , osati kudzikongoletsa ndi masitayilo omangila tsitsi , golide , ngale , kapena zovala zamtengo wapatali . ” Bungwe la UNHCR ( United Nations High Commissioner for Refugees ) linati masiku ano , “ munthu mmodzi pa anthu 113 ” padziko lonse “ ni wothaŵa kwawo . ” M’nkhani ino , taphunzila mmene Mkristu wofikapo kuuzimu angathandizile mpingo . Koma cifukwa ca khama la atumiki onse a Yehova , amene alipo mamiliyoni ambili , uthenga wabwino ukulengezedwa “ ku mitundu yonse . ” Cifukwa ca ucimo , kodi atumiki ambili a Mulungu amamvela bwanji ? “ MUNTHU wovutika ine ! ” Mau a Cigiriki amene Paulo anakamba amatanthauza ‘ kukonda wacibale . ’ ( Aheb . 6 : 1 ) Izi sizicitika zokha . Mwamuna wake sanafune kuti Marilyn apite . Koma ngati tagonja ndi kucita zimene io afuna , kodi angazindikile bwanji kuti zinthu za kuuzimu ndizo zofunika kwambili ? ” — Yelekezelani ndi 1 Petulo 3 : 1 , 2 . MUZIDALILA MULUNGU Zioneka kuti buku la Yakobo inalembedwa patapita nthawi yocepa Paulo atalemba za cikhulupililo . Koma Yehova na Mwana wake wokondedwa , adzatithandiza ndi kutipatsa nzelu kuti tikwanitse kuphunzitsa ena . ( Salimo 64 : 3 ) Ambili amaphunzila kukamba mwanjila imeneyi cifukwa coonelela mafilimu kapena mapulogalamu ena a pa TV . Komabe , iwo amatengela cikhulupililo colimba ca Sara , cikondi , na kuleza mtima kwake . Ine na amuna anga tinamvela monga kuti Yehova akutiuza kuti , ‘ Nili na imwe kuti nikuthandizeni pa mavuto anu . ’ Baibo imatilimbikitsa kuti : ‘ Mutulileni nkhawa zanu zonse , pakuti amakudelani nkhawa . ’ ( 1 Pet . A Zimba : Inde , Baibulo lanena kuti “ Wam’mwambamwamba ndiye wolamulila wa maufumu a anthu . ” Kodi Yehova amaŵaona bwanji Akristu okalamba ? Tingaŵelengenso Genesis 3 : 19 , limene limanena za cilango cimene io anapatsidwa pambuyo pocimwa , koma silimanena zopita ku moto wa helo . Kodi anthu a Mulungu ena akale anali kupeza bwanji ndalama na zinthu zina zimene anali kupeleka ? “ Njila ndi iyi . Tinali kukambanso kuti anthu akalandila uthenga wabwino umene tawalalikila , ndiye kuti aikidwa cizindikilo . Tsiku lina , abwana ake akale anam’tumila foni Blessing . Joel Dellinger Pamene anatuluka m’ndende , Rudolf anakhala na mwayi wotumikila monga woyang’anila dela . Pambuyo pake anaitanidwa ku Sukulu ya Giliyadi . Poona zimenezi , akulu - akulu a chechi anada nkhawa kwambili . Kuŵelenga Malemba olembedwa m’cinenelo cosavuta kwandithandiza kum’dziŵa bwino Yehova . Iye ali monga atate anga amene andifungatila m’manja ao ndi kundiŵelengela mau otsitsimula . ” M’BALE Lije anati : “ Pamene nkhondo yapaciweni - weni inayamba m’dziko la Burundi , banja lathu linali pa msonkhano wadela . Anthu amene anagwilizana ndi mipingo imene inakhazikitsidwa m’nthawi ya atumwi , anapindula kwambili ndi khama ndi kudzipeleka kumene oyang’anila ndi atumiki othandiza anasonyeza . ( Afil . 1 : 1 ; 1 Pet . Sitifunanso kuyambitsa mavuto pakati pa abale mumpingo . Tiyeni tikambilane za udindo wake wochulidwa m’Baibo . 26,060 Ndodo zimenezi zinafunika kukhala “ ndodo imodzi ” m’manja mwa Ezekieli . — Ezek . 2 : 7 . “ NYAMUKA , PITA . . . Kodi Sauli anakhala bwanji ndi mtima wodzikonda ? Tidziŵa bwanji kuti kukhala Mkhiristu kumafuna zambili kuposa kuleka cabe kucita macimo aakulu ? Yehova anabwelezanso lonjezo lake kwa Abulahamu , koma sanakambepo za Sara . — Genesis 13 : 14 - 17 ; 15 : 5 - 7 . ( a ) Ni mfundo iti ya pa Aroma 15 : 1 , 2 imene ingakuthandizeni kudziŵa zimene zingathandize ana anu ? Koma Hana anakhalabe wodziletsa , ndipo anayankhabe mwaulemu kwa Eli . Baibo imati : “ Basa atangomva zimenezi , nthawi yomweyo anasiya kumanga Rama n’kuimitsa nchito yake . ” Ena anasamukila kumalo osoŵa m’dziko lao . Izo zinali zosatheka . “ Simukudziŵa tsiku limene Ambuye wanu adzabwele . ” — MAT . Iye anacotsa mafano ndi mahule aamuna a pakacisi m’dziko la Yuda . ( 1 Akor . 13 : 4 , 5 ; ŵelengani 1 Petulo 4 : 8 . ) 7 : 3 , 5 ) Iwo analibenso nthawi yolambila Yehova pamodzi ndi mwana wao . Kodi tingathandize bwanji anthu kulemekeza Mau a Mulungu pamene tifuna kuwaŵelengela Baibo ? Pamene Yesu anauza otsatila ake kuti anyamule malupanga pa usiku wotsiliza wa moyo wake padziko , colinga cake sicinali cakuti awaseŵenzetse podziteteza . Yohane anachula Mkhristu wina dzina lake Demetiriyo kuti ni citsanzo cabwino . Iye anali wosiyana ndi Diotirefe . * Ndiyeno mu 70 C.E . , gulu lina la asilikali aciroma linapita ku Yerusalemu ndi kuononga mzindawo . Apo n’nali na zaka 10 . Kuyambila nthawi imeneyo , ine na amayi tinayamba kuyendela pamodzi mu ulaliki nthawi zonse . Iye anakamba kuti “ analimbikitsidwa ndi kutonthozedwa kwambili ” poona abale odzipeleka ocokela m’madela osiyana - siyana a ku Japan ndi a kumaiko ena . ( 2 Timoteyo 2 : 19 ) Mosiyana ndi Yehova , abale oŵelenga anthu amene amadya mkate ndi kumwa vinyo pa Cikumbutso sadziŵa kuti odzozedwa enieni ndi ati . MAKOPE 107,300,000 Caka cino , Cikumbutso ca imfa ya Yesu cidzakhalako pa Cisanu , April 3 dzuŵa litaloŵa . Iwo ndi alaliki komanso aphunzitsi aluso ndipo amauzako ena mumpingo zimene anaphunzila . Cilamulo ca Mulungu cinati : “ Munthu akacita cimo , mboni imodzi si yokwanila kutsimikizila kuti wacitadi colakwaco kapena cimo lililonse . Yehova ndi woceleza , amapatsa moolowa manja kwa onse ndipo amafuna kuti olambila ake azicita cimodzimodzi . Mosiyana ndi anthu akuthupi , anthu auzimu amayesetsa kutsatila miyezo ya Yehova pa zocita zawo zonse . ( Sal . Carl , mkulu amene anabatizika zaka zoposa 50 m’mbuyomo anati , “ Nimayesetsa kuona zizindikilo zilizonse zoonetsa kuti munthu ni woona mtima , monga kumwetulila , nkhope ya ubwenzi , kapena funso locokela pansi pa mtima . ” Debora na Baraki anayamba nyimbo yawo yacipambano ndi mau awa : “ Cifukwa ca kudzipeleka mwaufulu kwa anthu , tamandani Yehova . ” Anthu odwala amatonthozeka ngati wam’banja lawo wawagwila dzanja na kukamba nawo mokoma mtima . Tingaphunzilenso matanthauzo a mau ena amene sitiwadziŵa bwino . Mtumwi Paulo analembela Akhristu anzake kuti : “ Cititsani ziwalo za thupi lanu padziko lapansi kukhala zakufa ku dama . ” ( Akol . Abale a kum’mawa kwa Europe anali kusindikizanso mabuku m’maiko ao pogwilitsila nchito makina ocitila fotokope . Kamwalako n’kakang’ono kwambili kuposa kanjele ka thelele lobala , ndipo sikapezeka - pezeka . Ndipo ngati zoona ndife “ odzipeleka kwa Mulungu , ” tidzakhala okhutila ndi zimene tili nazo monga “ cakudya , zovala ndi pogona . ” — 1 Tim . 6 : 6 - 8 ; ftn . Pamene anthu a Yehova anayamba kulalikila ku United States , zinali zovuta kwambili kuyenda mitunda yaitali . Tifunikanso kukhala pa ubwenzi wolimba ndi anthu ena . Iye na mwamuna wake wokondeka , Abulahamu , anali atakhala zaka zambili mumzinda wa Uri , ndipo anali kusangalala . John anakhumudwa ngako na zimene wansembeyo anacita cakuti anamuuza kuti : “ Sinidzapondamonso phazi m’chechi ya Akatolika . ” Ambili a ise timakumbukila msonkhano wacigawo umene unatisangalatsa ndi kutilimbikitsa kukhala wacangu , ndiponso kukonda kwambili Mulungu wathu wamkulu ndi Mfumu yake . Yesu anacenjeza amunawo kuti ayenela kupitiliza kukhala okhulupilika . 7 , 8 . ( a ) Kodi kholo lina lacikhristu limaonetsa bwanji kuleza mtima pophunzitsa mwana wake ? Timaponya zopeleka zathu mosadzionetsela m’bokosi ya m’Nyumba ya Ufumu , kapena tingapeleke kupitila pa jw.org . M’malomwake , ni njila imene timakambila na Mlengi wathu . Mau a Mulungu amakambanso kuti zocita zathu zingacititse kuti tikhale na moyo wautali kapena waufupi . M’malomwake , tiyenela kuyesetsa kukondweletsa Yehova . Malemba amati cuma ca munthu wolemela ‘ m’maganizo mwake cili ngati mpanda woteteza . ’ ( Miy . Iwo anali kumuzonda kwambili cakuti anamugulitsa monga kapolo , ndipo anthu amene am’gulawo anapita naye ku Iguputo . Ngati muyamba kuŵelenga Baibo ndi kupitiliza kutelo , inunso mudzakhala na umoyo wabwino ndiponso mudzamudziŵa Mulungu . Ifenso tifunika kuona ubale wathu na Yehova kukhala wamtengo wapatali ndi kuuteteza . Anthuwo anafunikila kumacita zinthu mwadongosolo paumoyo wao makamaka polambila . Kodi tingakanize bwanji ‘ zosangalatsa zosakhalitsa zaucimo ’ ? 2 : 17 , 18 ; 4 : 16 . ( Mateyu 5 : 5 ) Pambuyo pake mu ulaliki umodzimodziwo , Yesu anachula cimene cidzathandiza kuti anthu asapitilize kuononga dziko . Anne wa zaka za m’ma 40 , amatumikila ku Asia m’dziko lina limene nchito yathu ni yoletsedwa . Posapita nthawi , n’nasankha kubatizika , ndipo pa September 5 , 1941 , a Bill ananibatiza mu dilamu ya nsimbi imene munali madzi ocokela pacitsime . N’cifukwa cake Baibo imati , “ zinthu zonse zimene zinalembedwa kalekale zinalembedwa kuti zitilangize , zimatipatsa ciyembekezo cifukwa malembawa amatithandiza kupilila ndiponso amatilimbikitsa . ” Tifunika kuulula macimo athu kwa iye . Baibulo limaonetsa kuti Yesu anali kukonda Marita , ndipo anali mabwenzi abwino . Paulo analemba kuti : “ Nthawi yotsalayi yafupika . Ngati ndinu wokalamba ndipo mumadwaladwala komanso mphamvu zanu zikucepelacepela , mungakumbukile mau a pa Mlaliki caputala 12 . Mu April 1954 , n’nadzipeleka kwa Yehova na kubatizika . Inde , ndikudziŵa kuti mumandimva nthawi zonse . ” * — Yoh . 3 : 19 , 20 ; Sal . Nanga ni mbali ziti zimene nifunika kuwongolela ? ’ Nanga zolipila misa ya pamalilo , kapena kulipila misa ya apapa kapena abusa zinalembewa pati ? ’ Podzafika mu 1919 , anthu amene anali kutumikiladi Yehova pa kacisi wake wauzimu anadziŵika . Tiyeni tikambilane zina mwa zifukwa zimenezi . ( Dan . 1 : 19 , 20 ) Zikanacititsa kuti akhale wodzikweza ndi womva zake zokha . ( Yohane 3 : 16 ; 1 Yohane 4 : 9 , 10 ) Mtumwi Paulo anakamba kuti imeneyi ndi “ mphatso . . . yaulele , imene sitingathe n’komwe kuifotokoza . ” Mu 1987 , m’bale wina ananipempha kuti nikaonane ndi munthu winawake wacidwi amene anali kukhala m’tauni ya Balykchy . Nimapewa kuseŵenzetsa maluso anga pofuna cabe kudzipindulitsa kapena kupeza nchito yapamwamba . Koma sitikaikila kuti Yehova amathandiza onse amene amavutika cifukwa ca dzina lake . N’ciani cimene tikambilane ( a ) m’nkhani ino ( b ) m’nkhani yotsatila ? Abuda , Akatolika , Apulotesitanti , Ahindu , Asilamu ndi zipembedzo zina zimayesa kugwilila nchito pamodzi kuti zithetse umphaŵi , zibweletse ufulu wa anthu , ziletse kufocela mabomba kapena kusamalila zacilengedwe . “ Ngati munthu akufuna kunditsatila , adzikane yekha . ” — MAT . Otsatila a Yesu akugwila nchito imeneyi mwakhama , ndipo pa cifukwa cimeneci , anthu ambilimbili akubatizidwa caka ciliconse . Anthuwo amayamba kugwila nafe nchito yolalikila . Kuti tipeze yankho , tiyeni tikambilane za atumwi aŵili . Iwo amaphunzila kuti Abulahamu , Yobu , na Danieli anali kukhulupilila kuti m’tsogolo akufa adzauka . Popeza kuti cilungamo ca Mulungu ndi capamwamba kwambili , zinali zosatheka kuti anthu opanda ungwilo adziombole okha . N’cifukwa ciani tili otsimikiza mtima kuti cifuno ca Yehova sicidzalephela ? Davide anapitiliza kukamba motsimikiza kuti angakwanitse kugonjetsa Goliyati , ndipo munthu wina anapita kukauza Sauli zimenezi . Nyumba ya Ufumu ndi cimake ca kulambila koona m’dela lililonse . Iwo angakambe kuti anthu ambili amene anamwa mankhalawo anacila . Conco , kulibe cikwati cangwilo . N’nadziuza kuti , ‘ Zioneka kuti uyu ndiye mkazi amene ndidzamanga naye banja , pokhapo ngati cina cake calepheletsa . ’ Nawonso abale a ku Greece amapeleka mafuta a maolivi , chizi , ndi zakudya zina ku banja la Beteli . Mulungu anafuna kuti anthu akhale padziko lapansi kosatha ndipo iye adzakwanilitsa colinga cake . — Yesaya 55 : 11 . 2 : 13 ) Kodi Akhristu amitundu ina anacita ciani ataona zinthu zopanda cilungamo zimene Petulo anawacitila ? N’cifukwa ciani tifunika kuzidziŵa bwino nyimbo za m’buku latsopano ? Kuti cilengedwe cikhaleko Mlengi wake anafunika kukhalako coyamba . Ngati zinali conco , ndiye kuti kudzicepetsa kunawateteza . Kunawathandiza kupitiliza kulambila Yehova mokhulupilika , ali na cidalilo cakuti Mulungu wawo sangacite zinthu zosalungama . ( b ) N’ciani cimene omasulila Baibulo ambili acita ndi dzina la Mulungu ? ( Yohane 6 : 15 ; 17 : 16 ) Cifukwa cina n’cakuti timacilikiza Ufumu wa Mulungu . Conco , ngakhale tikuona kuti tinacita colakwa cacikulu , sitiyenela kuleka kupempha Yehova kuti atikhululukile . Baibulo silikamba , koma tidziŵa kuti Mdyelekezi anali kufuna kuipitsa Sara kuti akhale wosayenelela kubeleka mwana amene Yehova analonjeza . Kodi mungangocoka pa malowo ndi kupita kunyumba kukasintha zovala , ndi kuiŵalako za munthu amene wakupulumutsani ? Tiyenelanso kukhala osamala kwambili pankhani yotumila ena nkhani yokhudza abale athu , kapena zocitika zina zimene tamvela . Panthawiyo , panali ‘ magulu aŵili oimba nyimbo zoyamika ’ Mulungu . Potiyankha , anangotiuza kuti tipite ku Pine Bluff , m’dela la Arkansas . Ndipo Purisikila ndi Akula anaseŵenzetsa nthawi yawo ‘ kufotokozela [ ena ] njila ya Mulungu molondola . ’ Zikakhala conco , tiyenela kutsatila malangizo akuti : “ Muzicelezana popanda kudandaula . ” ( 1 Pet . Anthu enanso anali na mwayi woona kuukitsidwa kwa munthu wina . Kodi kudziŵa coonadi ndimakuona kukhala mwai wapadela ndiponso waukulu ? ’ 13 : 48 ) M’malo mokhala okhumudwa ndi nkhawa kwambili , io amakhala acimwemwe , ndipo amadalila Atate wathu wakumwamba . ( 1 Timoteyo 2 : 4 ) Motelo , zimene timakhulupilila zifunika kukhala zogwilizana ndi coonadi ca m’Baibulo . N’ciani cingatithandize kukhala odzicepetsa ? KODI mumamvela bwanji ngati munthu amene mumam’dziŵa na kum’lemekeza waiŵala dzina lanu , kapena ngati wakamba kuti sakudziŵani ? Mwacitsanzo , Yesu anakamba kuti : “ Odala ndi anthu amene amazindikila zosoŵa zao zauzimu , cifukwa ufumu wakumwamba ndi wao . ” — Mateyu 5 : 3 . Koma kucokela pa nthawiyi , tinayamba kuyenda tekha . Iye anadwala kwambili . Imeneyi ndi mfundo imene amatsatila . Tidzapeza mayankho pa mafunso amenewa mwa kukambilana za makonzedwe a mizinda yothaŵilako m’nthawi ya Aisiraeli . PONENA za Cikumbutso ca imfa ya Yesu cimene timacita caka ciliconse , kodi munaŵelengako Aroma 8 : 15 - 17 ? Boma la Mulungu , limene ndi Ufumu wa Mesiya , ndi umboni winanso wakuti Yehova amatikonda . Zimenezi zikadzacitika m’pamene cifunilo ca Mulungu cidzacitika padziko lapansi monga mmene zilili kumwamba . Ngati tiyesetsa kucita zinthu zabwino , Mulungu adzatikonda na kutiteteza , ndipo sitidzalandila tembelelo la imfa . Kwa zaka zambili , iye anali kukopeka ndi alongo ena koma io sanali kum’konda . Conco , n’zokayikitsa kuti iye anaona pamene Yesu anaukitsa mwana wa mkazi wa masiye , amene anali kukhala kufupi na mzinda wa Naini , ku Galileya . Limanenanso kuti : “ Zinthu zonse zinakhalako kudzela mwa iye , ndipo palibe cinthu ngakhale cimodzi cimene cinakhalapo popanda iyeyo . ” 11 : 3 ) Lemba limeneli limalimbikitsa amuna kuti ayenela kutsatila mmene Kristu amacitila umutu wake kwa amuna . Yesu sanali kupondeleza anthu kapena kuwacitila nkhanza . “ Ana athu afunika kuona kuti zimene amatiuza timaziona kukhala zofunika . 9 : 31 ; 15 : 28 ; 2 Tim . 3 : 16 , 17 ) Malangizo ocokela kwa iye ndi osavuta kumva cakuti zimakhala ngati ‘ makutu athu akumva mau kumbuyo kwathu , akuti : “ Njila ndi iyi . Asanabwele padziko lapansi , iye anali “ mmisili waluso ” wa Mulungu , ndipo anali ‘ kusangalala ndi zinthu zokhudzana ndi ana a anthu . ’ ( Miy . 8 : 46 ) Ndiponso , kaya tikhale na nzelu kapena luso labwanji , tidzakhalabe monga ana kwa Yehova . — Yes . Yehova Ndi Bwenzi Lathu Lapamtima , 2 / 1 Yehova Mulungu nthawi zonse amafuna kuti tizimuuza zinthu zimene zikutivutitsa . Ndiponso pamisonkhano yampingo , tonsefe timalandila malangizo a panthawi yake . Pankhani imeneyi , mtumwi Paulo analemba kuti : “ Mawu a Mulungu ndi amoyo ndi amphamvu , ndipo ndi akuthwa kuposa lupanga lililonse lakuthwa konsekonse . “ Nimakonda kugona mwamsanga , koma makambilano ena abwino amene nakhalapo nawo ndi ana anga acicepele , anacitika capakati pausiku . ” — Herbert . Kaya zosankha zanu n’zotani , muyenela kugwila nchito inayake kuti muzipeza zofunika pa umoyo wa tsiku ndi tsiku . Ngakhale n’conco , tifunika kudziŵa mayankho pa mafunso atatu ofunika kwambili aya : Kodi mphamvu za Satana n’zazikulu bwanji ? Tandifotokozelani malotowo . ” Msonkhano utatha , kunagwanso cimvula . Nimakondwela kuceza ndi acicepele a mu mpingo wathu Fanizo la matalente ndi limodzi mwa mafanizo anai opezeka pa Mateyu 24 : 45 mpaka 25 : 46 . Anthu ena odzicha kuti ndi Akristu anatengela ziphunzitso zonyenga . 8 , 9 . ( a ) Ni mfundo ziŵili ziti zimene taphunzilapo pa citsanzo ca Adamu , Hava , na angelo opanduka ? Cioneka kuti mauwa amakamba za munthu wogwila nchito ya m’munda amene anali kum’ganizila kuti analephela kusonkhanitsa mbewu zonse zimene anauzidwa kuti asonkhanitse . Mau ake ni akuti : “ Ine mtumiki wanu [ wodandaula ] nitatsiliza kusonkhanitsa mbeu masiku angapo apitawo , Hoshayahu mwana wa Shobayi anabwela n’kutenga covala canga . . . . 20 : 5 , 6 ) Komabe , amene adzaukitsidwa kuti adzakhale ndi moyo padziko lapansi adzaphatikizapo “ osalungama . ” ( Mac . Ndipo anali kukakamizidwa kucitako zimenezo . Kodi colinga ca Yehova potiyang’ana cimasiyana bwanji ndi colinga ca anthu pogwilitsila nchito makamela ? M’maiko ambili masiku ano , kusankhila munthu wokwatilana naye kumaoneka kwacilendo . Muzisinkhasinkha zimene mwaŵelenga . Conco , ndinayamba kucita zinthu zoipa kwambili . ( Miyambo 3 : 9 ) Timacita zimenezi mwa kum’lemekeza pogwilitsila nchito zinthu zimene tili nazo . Kuwonjezela pa zitsanzo za m’Malemba , pali zitsanzo zina zambili zamakono za atumiki a Mulungu okonda zinthu zauzimu , amene amayesetsa kutengela makhalidwe a Khristu . Koma tsopano n’cowonongeka kwambili cakuti mawu ambili anafutika ngakhale kuti papita zaka zosakwana 250 . Mungatengele citsanzo ca Yesu ca mmene anali kuphunzitsila ophunzila ake mwacikondi , modzicepetsa , ndiponso mozindikila . 13 : 10 - 14 ) Ici ndiye cinali ciyambi ca masoka amene pothela pake anam’tayitsa ufumu wake . Koma coipilatu n’cakuti anakaniwa na Yehova . ( 1 Akor . 13 : 4 ) Kuti nsanje isazike mizu mu mtima mwathu , tifunika kuyesetsa kuona zinthu mmene Mulungu amazionela . Tiyenela kukumbukila kuti ise na Akhristu anzathu ndise ziwalo za thupi limodzi . Pa nkhani ya dipo , malipilo ake ayenela kulingana na cinthu cimene cinawonongedwa . Atumiki a Yehova ambili masiku ano ali mbali ya “ khamu lalikulu . ” Iwo amacokela m’madela osiyanasiyana kuzungulila dziko lonse , ndipo amacilikiza Ufumu wa Mulungu . Tifunika kukumbukila ciani pankhani yaucimo ? Ngati inunso mukumana na vuto laconco , dzifunseni kuti : ‘ Kodi mwamuna kapena mkazi wanga akuniletsa kulambila Mulungu ? Kumbukilani kuti : Yesu ‘ anapita kukagonjetsa ’ mu 1914 . Kodi tinganene kuti munthu ayenela kusankha kukhulupilila Yesu kapena Yehova ? Wa m’banja akacotsedwa mumpingo kapena akadzilekanitsa , zimapweteka kwambili mumtima cakuti munthu angamvele monga walasiwa na lupanga . Anavomeleza kuthandizidwa na Hananiya , wophunzila wa Khristu . Colinga ca Yehova pamene analenga anthu kudzela mwa Yesu cinali cakuti adzaze dziko lonse . ( Gen . Ndipo iwo anali kuphunzitsa anthu m’kacisi nthawi zambili . Ndiye cifukwa cake kuona mabwenzi a Mulungu monga adani athu kungakhale kulakwitsa kwambili . — Salimo 141 : 5 . Mulungu wacilungamo salephela kulanga anthu oipa panthawi yake yoyenela ndipo amaweluza mwacifundo ngati n’koyenela kutelo . Pamene tikukambilana fanizo lililonse , tiyenela kupeza mayankho a mafunso awa : Kodi fanizo limeneli limatanthauza ciani ? CRISTINA , mtsikana wa zaka 18 anati : “ Makolo anga sanilimbikitsako olo pang’ono . 9 : 7 ) Mlongo wina wa ku Canada dzina lake Catherine , amasangalala kwambili kuyang’ana cilengedwe , makamaka m’nyengo imene zinthu zimaphukila . Tingaonetse bwanji kuti timakonda abale ? Iye ananena kuti kulambila mwana wa ng’ombeko cinali “ cikondwelelo ca Yehova . ” Kwa nthawi yaitali ndithu , iye ayenela kuti anali kuona zithunzi m’maganizo ake za mavuto amene anakumana nawo . Napeza mapindu ambili cifukwa cotsatila malangizo a m’Baibo , ndipo niona kuti n’tawalemba , angadzale m’buku . Onse anakhudzidwa ndi mwambo wakale kwambili wa kuba anthu , n’colinga cakuti awacite malonda ndi kupezelapo ndalama basi . M’malo mwa milili na imfa , anthu onse adzakhala na thanzi labwino komanso moyo wosatha . Kalata yaciŵili , imene analemba patapita miyezi ingapo , ionetsa kuti kuwongokela kunalipo , kutanthauza kuti akulu anatsatila malangizo a Paulo . 2 : 17 . Izi zawathandiza kuzindikila zilakolako zoipa zimene zingayambe m’mitima yao , ndi kuongolela maganizo amenewo . — Sal . Amayi anali akhama pa nchito yolalikila uthenga wabwino ndipo anali kucititsa maphunzilo a Baibo ambili kwa anthu acidwi . 1 : 22 . Mofanana ndi atumwi , atumiki a Yehova a masiku ano amacitanso cidwi ndi fanizo limeneli cifukwa limakhudza tsogolo la anthu . Iwo ali ndi udindo wolela ana ao “ m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake . ” ( Aef . Ndinali kuyesetsa kuuzako anthu a m’banja langa coonadi . Conco , Mulungu anawadalitsa ndipo anakhala ndi mabanja aoao . — Eks . N’cifukwa ciani kulimbikitsana kudzakhala kofunika ngako m’tsogolomu ? Nanga tifunika kucita ciani ? Pamene tipilila pa nchito yolalikila , timakhala na mtendele waukulu wa mumtima , umene umabwela cifukwa codziŵa kuti ndise oyanjidwa na Yehova na Yesu . ( Sal . Kaŵili - kaŵili , ine na Mairambubu tinali kupita ku Balykchy . Koma ngakhale kumaiko amenewo , abale ena angasankhe kusasunga ndevu . Rico atafika zaka 12 , anabatizika . ( Maliko 3 : 35 ) Colinga ca Mulungu n’cakuti “ khamu lalikulu ” limene silidziŵika ciŵelengelo , locokela m’dziko lililonse , fuko lililonse , ndi cinenelo ciliconse , likhale olambila ake . ( Luka 22 : 36 - 38 ) Usiku wa tsiku limenelo , Petulo anatenga lupanga na kutema nalo mmodzi wa anthu amene anabwela kudzagwila Yesu . ( Miyambo 2 : 1 - 5 ) Maganizo a anthu amasinthasintha , koma Yehova sasintha . Mumtima cinaniwawa kwambili cakuti n’nafuna kubwezela , koma n’nathawa cabe . Ndiyeno , patapita wiki imodzi , tinaitanidwa kuti tipite ku maphunzilo a nchito ya m’dela . Ndipo tinatumikila monga oyang’anila dela kumpoto kwa Ontario kwa zaka ziŵili zotsatila . “ Tsiku lina mwamuna wanga anapepesa pa zimene anacita zonikhumudwitsa kwambili . Ngati mumatangwanika na zinthu monga TV kapena foni , mungacite bwino kuzimya TV na kuika foni pambali . M’malanga , adokowe ena oposa 300,000 amacoka ku Africa kupita kumpoto kwa Europe kudzela m’cigwa ca Yorodani . ( Aroma 5 : 12 ) Ndipo zotsatilapo zake zoipa ndi kutaikilidwa okondedwa athu mu imfa , monga atate wanga . ( Afilipi 4 : 13 ) Patapita nthawi , ndinaleka kukoka fodya . — 2 Akorinto 7 : 1 . Mphamvu imene tili nayo yotha kuganizila zinthu zimene sitinazionepo tingaigwilitsile nchito mwanzelu kapena molakwika . Mwamunayo anali kuoneka kuti ndi wokoma mtima . Kumvetsetsa mbili ya gulu lathu kwatithandiza kuzindikila bwino zocitika zina zolembedwa m’Baibo . N’nakulila m’banja la alimi osauka , ndipo n’naphunzila kwa zaka 5 cabe . Koma tidzapeza njila yokukhaulitsilani , mudzaciona ! ” Mwacitsanzo , m’nthawi yocepa cabe munthu angaŵelenge ndi kumvetsetsa buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni . 4 : 5 , 6 . “ Musakalipe , olo kuti zimene mwana wanu aganiza n’zolakwika . ” — Anthony . Cosankha cimene Sara anafunika kupanga cingaoneke cacilendo kwa ife . Muziŵelenga muli ndi maganizo oyenela . Yehova amawakonda kwambili anthu okhulupilika ( Onani palagilafu 14 , 15 ) Koma ngati timacita zoyenela ndi kuika zinthu za Ufumu patsogolo mu umoyo wathu , tisakaikile kuti Yehova adzatipatsa ciliconse cimene tifuna . A Inoki : Conco , vesi limodzi lokha limeneli la m’Baibulo , ngakhale kuti linalembedwa zaka pafupifupi 2,000 zapitazo , likufotokoza zimene mwamuna ndi mkazi afunika kucita . Phunzitsani Ana Anu Acinyamata Kutumikila Yehova Kuwonjezela apo , nkhani ya m’Genesis imachula za mitsinje inayi yocokela m’mundawo . 12 : 22 ) Kodi anatanthauza ciani ? Yesu ndi angelo ake anacotsa Satana ndi ziwanda zake kumwamba . Wamasalimo anati : “ Wodala ndi aliyense woopa Yehova , amene amayenda m’njila za Mulungu . ” Anthu amene anapulumuka , monga Baruki ( mlembi wa Yeremiya ) , Ebedi - meleki Mwiitiyopiya , ndi Arekabu , sanali ndi cizindikilo ceniceni pamphumi pawo . M’bale wina anayembekezela kwa zaka zoposa 10 asanakhale mkulu . Ngakhale kuti n’zosatheka kuti mudziŵe zimene zili mumtima mwa munthu mofanana ndi Yesu , mukhoza kukhala wozindikila . Ndithudi , Yehova anapambana koma Satana analephela . Komanso Baibulo lingakuthandizeni kukhala ndi ciyembekezo camphamvu pa malonjezo a Mulungu . Tinamasulilanso buku lakuti Choonadi Chimene Chimatsogolera ku Moyo Wamuyaya m’Cituvalu , ndi kulisindikiza ndi makinawo . Akristu sayenela kulola tsankho kuwacititsa kuona anthu ena molakwika . Tiyeni tikambilane uthenga wofunika womwe uli m’fanizo la Yesu limeneli . Inde , angapambane , ndipo akupambana kumene ! ( Yoh . 6 : 40 ) Cifukwa ca cikondi ndi nzelu zake , Yehova adzathandiza banja la anthu kukhala langwilo , monga mmene anali kufunila poyamba . Kukonda Mulungu ndi anthu , komanso pakuti nchito yolalikila Ufumu ifunika kucitika mwamsanga , anthu a Mulungu ‘ akupeleka mphatso kwa Yehova ’ mwa kucita zopeleka zaufulu . ( 1 Akor . Wolemba wina ananena kuti : “ Akazi a asodzi sakanatha kupeleka cinthu codula ngati cimeneco . ” — Yoh . 19 : 23 , 24 . Baibulo limalangiza anthu amene amafuna ‘ kuyandikila Mulungu ’ kuti : “ Yeletsani manja anu , . . . ndipo yeletsani mitima yanu . ” M’nthawi yocepa kunakhadzikitsidwa mpingo wocita bwino . Baibulo Inapulumuka kwa Anthu Otsutsa 5 Iwo amagwila nchito mwakhama pothandiza akulu , ndipo timawayamikila pa zonse zimene amacita . Kodi mumacita naye bwanji zinthu mnzanu wa m’cikwati komanso ana anu ? Olo kuti zimakhala zovuta , anthu ambili acikondi amapitiliza kusakila mphatso yoyenelela imene angapatse munthu wina amene amamukonda kwambili . ( 1 Petulo 5 : 7 ) Iye akukupemphaninso kuti muzimuuza mavuto anu . Satana ndi ziŵanda zake ali kumbali imodzi , akuona mavuto amene mukukumana nao , ndipo akukamba kuti mugonja . Ngakhale kuti tinali kukumana na mavuto amenewa , tinapitiliza kugwila nchito yolalikila ku Armavir . Komabe , Baibo imalimbikitsa Akhiristu kukhala ofatsa . Ni malemba ati amene angatonthoze anthu ofedwa ? Okalamba ena amasunga khadi lao la DPA pamodzi ndi wilo , zipepala zina zofunika za inshuwalansi , za ku banki , ndi manambala a maofesi a boma othandiza okalamba . ZIMENE MUNGACITE ZINTHU ZIKASINTHA Ganizilani kugwilizana kwa mavesi a m’nkhani imene muŵelenga Lemba limeneli linam’kumbutsa kuti kukondweletsa Yehova ndico cinthu cofunika kwambili . M’mipingo yambili mungasowe abale oyenelela amene angamasamalile maudindo mumpingo . ( b ) Kodi mtundu watsopano unakula motani m’nthawi ya atumwi ? Kodi ndi liti pamene tidzafunika kukhala ogwilizana kwambili ? ( Ŵelengani 1 Petulo 1 : 8 , 9 . ) ( Aroma 8 : 38 , 39 ) Atumiki a Yehova akamwalila sizitanthauza kuti Satana wapambana cifukwa Yehova adzaonetsetsa kuti onse aukitsidwa . Iwo anali kuimba nyimbo , kupemphela , ndi kukambilana Malemba . LMofanana ndi William ndi Jennifer , Megan , mlongo wosakwatiwa wa ku United States , nayenso akutumikila monga mpainiya . Iye ‘ akukondwela ndi utumiki wake ’ pamene akuyesetsa kuphunzila bwinobwino cinenelo ca Cichaina . Ndipo maphunzilo ocokela kwa Yehova angapulumutse moyo wao . Onani zinthu zitatu zimene zimapangitsa anthu kusamvetsetsa Baibo . ( Aheb . 10 : 36 ) Koma n’ciani cingakuthandizeni kupilila ? N’cifukwa ciani makolo ena amafuna kuti ana awo asabatizike mwamsanga ? Komanso tikakhala okhulupilika , tidzakhala na tsogolo labwino . — Deut . Iye amatsogolela anthu ake n’colinga cakuti adzapeze moyo wosatha ndiponso kuti apewe mavuto . Mu ulamulilo wa Kristu wa zaka 1000 , a khamu lalikulu adzakondwela kufotokozela anthu amene adzaukitsidwa mmene zinalili kukhala Mboni ya Yehova m’masiku otsiliza . Nkhani yapita m’magazini ino inafotokoza kuti anamwali amaimila ndani . Ine na Nora timamuyamikila ngako Yehova pa zinthu zonse zabwino zimene watipatsa , ndipo timalimbikitsa ena kuti amuyese Yehova . — Mal . 15 , 16 . ( a ) N’cifukwa ciani tiyenela kuyang’anitsitsa pamphoto yathu ? Iwo safunika kudziŵa maina a odzozedwa onse kuti ayambe kuwatsatila . Mwacionekele , Timoteyo ndi Akristu ena anada nkhawa kwambili ndi zocita za ampatuko anali pakati pao . Ndipo salankhula mau aukali , odzudzula nthawi zonse , kapena onyoza . Mwacitsanzo , anasankha mtundu wa Aisiraeli kukhala anthu a dzina lake , ndi “ cuma cake capadela . ” ( Deut . 3 Anadzipeleka Mofunitsitsa ku Micronesia ( Genesis 2 : 17 ; 3 : 1 - 6 ) M’mau ena , Satana anakamba kuti anthu akhoza kudzilamulila bwino popanda Mulungu . ( Genesis 39 : 21 - 23 ) Cifukwa cakuti Yosefe anali kugwila nchito mwakhama , Mulungu anapitilizabe kumudalitsa . Iye sanalakwitse . Kodi Yehova anathandiza bwanji Kaini ndi Baruki ? Kodi anali kukonda kwambili nsomba ndi bizinesi ya nsomba kuposa mmene anali kukondela Yesu ndi zinthu zimene anam’phunzitsa ? Ngati anali ndi zaka zakubadwa zofanana ndi Yesu kapena kuposelapo pang’ono , ndiye kuti pamene anakumana ndi atumwi ena ku Yerusalemu mu 49 C.E anali ndi zaka pafupi - fupi 50 . Koma cifukwa ca kupanda ungwilo , tikhoza kuona zinthu molakwika . Baibulo limayelekezela uthengawo ndi matalala pamene limati : “ Matalala aakulu , lililonse lolemela pafupifupi makilogalamu 20 , anagwela anthu kucokela kumwamba . Anthuwo ananyoza Mulungu cifukwa ca mlili wa matalalawo , pakuti mliliwo unali waukulu modabwitsa . ” — Chiv . “ Mulungu si wosalungama woti angaiŵale nchito yanu ndi cikondi cimene munacisonyeza pa dzina lake . ” — AHEB . Anthu a Yehova “ Aleke Kucita Zosalungama ” 4 : 5 ) Kodi n’ciani cimene tidzalalikila kwa anthu ? Komabe , n’nali kuphunzitsa timu ya kufupi ndi kwathu za maseŵela amenewa . Nthawi zina akuluakulu a boma amaba katundu wa boma , ndalama , kapena kuuza anthu ena kuti awacitile zinazake zimene sayenela kuwacitila . Tidziŵa bwanji kuti nthawi zina kusintha zosankha zathu kuli cabe bwino ? Misonkhano imatithandiza kukhala ogwilizana monga anthu a m’banja limodzi amene amakondana . M’nyengo yotentha , misonkhano tinali kucitikila kusanga . Ngati ‘ tinyalanyaza colakwa , ’ Yehova amakondwela kwambili . ( 1 Akor . 11 : 3 ) Koma kodi n’zinthu ziti zimene mutu wa banja ayenela kuganizila asanapange cosankhaci ? Tinayetsesa kuwathandiza kudziŵa ubwino wopewa kukwatiwa akali aang’ono . Ndipo nchitoyi inali kufunika kucitidwa mwamsanga . Zimenezi zapangitsa kuti anthu ambili akhale ndi Baibulo la Dziko Latsopano m’cinenelo cao . Kale , iye analanga anthu ena mwa kuwadwalitsa . Mabaibo amenewa sanafalitsidwe ndipo sangapezeke . M’nkhani ino , tidzaphunzila cifukwa cake timakhulupilila kuti Yesu anaukitsidwa ndipo ali moyo . Mafunso otsatilawa adzatithandiza kudzifufuza . Posacedwa Ufumu umenewu udzapangitsa cifunilo ca Mulungu kucitika pa dziko lonse . KULEMEKEZA munthu kumatanthauza kumuona kukhala wofunika ndi kum’patsa ulemu . Pali mipata yambili yotumikila Yehova . ( Ŵelengani 1 Akorinto 3 : 9 . ) Mavuto amene timakumana nawo amakhala osiyana - siyana . Ndiye cifukwa cake anacita zilizonse zimene akanatha kuti anthu onse akhale na Baibo . ‘ Mwa kukonda Mulungu , kumvela mau ake ndi kum’mamatila . ’ MFUNDO YA M’BAIBO : “ Kuganiza bwino kudzakuyang’anila , ndipo kuzindikila kudzakuteteza . ” — Miyambo 2 : 11 . ( Aroma 13 : 8 - 10 ) Conco , tiyenela kupitilizabe kukonda anzathu . Nanga cikhulupililo ca Timoteyo cingatilimbikitse bwanji ? Ngati Mboni zacikuda zilalikila ku nyumba ndi nyumba m’dela lokhala azungu , zinali kumangidwa komanso nthawi zambili zinali kumenyedwa . Nkhaniyi imanena kuti , “ akazi onse aluso anawomba nsalu ndi manja ao . ” Jumpei anati : “ Kuyambila kale - kale , ine na mkazi wanga tinali na colinga cokatumikila m’gawo losoŵa ku dziko lina . Ndipo imeneyi ni nkhani ya moyo kapena imfa . Ngakhale n’conco panali zina zovuta . Popeza kuti kudzakhala anthu abwino okha - okha , dziko lapansi lidzakhala paradaiso . 4 : 7 ) Tsiku lotsatila , msilikali wina wokoma mtima ananipatsa cakudya , madzi , ndi cikhoti . Zimene zidzacitika mtsogolo zidzakhala zosiyana kwambili ndi zimene anthu ambili amalosela . Liu lacingelezi lomasulidwa kuti “ cinyengo ” linacokela ku liu la cigiriki limene limakamba za ocita maseŵelo amene kaŵilikaŵili amadzibisa nkhope kuti anthu asawadziŵe . Ayi , koma anali asanafike pa msinkhu woloŵa usilikali , ndipo ayenela kuti anali kuonekabe wacicepele . Tiyenela kukumbukila kuti nayenso ni munthu wopanda ungwilo . Conco , n’zosavuta kuyamba kutengela maganizo ndi zocita za anthu a m’dzikoli . Mwamuna wina dzina lake Katsuo Miura ndi mkazi wake Hagino , anapatsidwa mabuku ndi Mlongo Ishii . Komabe , iye anali na cidalilo cakuti angapambane nkhondoyo mwa kupemphela kwa Yehova ndi kukhulupilila nsembe ya dipo la Yesu . Mfundo za m’Baibo ni ‘ mfundo za coonadi zofunika kwambili kapena ziphunzitso zimene zimatitsogolela popanga zosankha kapena kucita zinthu . ’ 1 : 8 ) Koma kodi akanaikwanitsa bwanji nchito yaikulu imeneyo ? Ana aakazi a Salumu anathandiza pa nchito iti ? Nanga alongo masiku ano amathandiza pa nchito yofananako iti ? “ Yamikani Yehova , cifukwa iye ndi wabwino . ” — SAL . Kutumikila pamodzi na M’bale Knorr unali mwayi waukulu . Golide imeneyo imakhala mkati mwa miyala , ndipo amafunika kukumba ndi kuphwanya miyalayo kuti atengemo golide . Ngati ndi conco , dziŵani kuti ndinu wofunika kwambili m’gulu la Yehova la padziko lonse . Poyamikila mlongo amene alibe mwamuna , tingamuchulile zimene zimatikondweletsa tikaona mmene akulelela ana ake ngakhale kuti zinthu n’zovuta mu umoyo wake . Ngati tili na cikondi camphamvu kwa Mulungu na munthu mnzathu , sitidzalola munthu kapena cinthu ciliconse kusokoneza cikwati cathu . Ndiyeno anaponya kapolo woipa uja “ kunja kumdima , ” ndipo kumeneko analila ndi kukukuta mano . — Mat . yacingelezi mmene munali nkhani zakuti “ Understanding Your Doctor ” [ Kudziŵa Bwino Dokotala Wanu ] mu maofesi oposa 100 a madokotala m’dela lake . Malinga n’zimene Baibo imakamba , kodi munthu wakuthupi na munthu wauzimu amasiyana bwanji ? Mosiyana na mavuto amene munthu amapeza cifukwa cokhala ku mbali ya Satana , ganizilani madalitso amene muli nawo cifukwa cokhala Mkhristu wodzipeleka na wobatizika . M’malo mongomufotokozela mfundo cabe , mungamuthandize kuyelekeza m’maganizo zocitikazo . ( Yoh . 5 : 28 , 29 ) Palibe ciliconse cimene tingapeze m’dziko loipali cimene cingalingane na mwayi wogwila nchito pamodzi ndi amuna ndi akazi okhulupilika potumikila anthu a Mulungu padziko lonse lapansi . ( 1 Pet . 3 : 1 ) Mau amenewa amanena za akazi acikristu , koma amagwilanso nchito kwa amuna amene anakhala Mboni ali kale okwatila . Iye “ anapita ku Yerusalemu kukapembedza Mulungu . ” — Machitidwe 8 : 27 . 2 : 44 - 47 ; 5 : 42 ) Ngakhale zinali conco , ena mwa otsatila a Yesu a m’zaka 100 zoyambilila analola cikondi cawo kuzilala . Titafika kumeneko , mwamsanga tinapitiliza kucita zinthu zauzimu . Iye anati : Ndimakondwela kuŵelenga nkhani zokhudza maulendo cifukwa ndikamaziŵelenga zimakhala ngati ndapita kudziko lina . ” Nthawi zina , atumwi anali kuika abale mwacindunji . Mwacitsanzo , amuna 7 anawaika kuti aziyang’anila nchito yogaŵila cakudya ca tsiku ndi tsiku kwa akazi amasiye . 4 : 5 - 30 ) Anakambilananso ndi Mateyu wokhometsa msonkho , amene anali kuchedwanso kuti Levi . Anthu ambili amacita cidwi akaona kuti dzina la Mulungu likuchulidwa nthawi zambilimbili m’mipukutu yakale . Kuti tipindule na malamulo a Mulungu , tifunika kucita zambili osati cabe kuyaŵelenga kapena kuyadziŵa . Usacite mantha kapena kuopa , pakuti Yehova Mulungu wako ali nawe kulikonse kumene upiteko . ” — Yos . ( Ŵelengani 1 Yohane 4 : 9 , 10 , 19 . ) Yesu anayenda kukaona apongozi a Petulo ndipo anawacilitsa . — Mateyu 8 : 14 , 15 ; Maliko 1 : 29 - 31 Kuposa wina aliyense , Yehova angakuthandizeni kupanga zosankha mwanzelu mukali acinyamata . [ Cithunzi papeji 20 ] Atumiki ambili a Yehova apewa mavuto mwa kumvetsela kwa Yehova pamisonkhano . Kodi cakudya ca kuuzimu cimene timalandila pa misonkhano yadela ndi yacigawo cimaonetsa bwanji kuti Yehova ndi Bwenzi lathu ? Tiyenela kumvetsa zimene fanizoli limatanthauza , cifukwa cakuti limakhudza Akristu onse oona , kaya akuyembekezela kudzalandila mphoto yao kumwamba kapena padziko lapansi . Kodi Baibulo lionetsa bwanji kuti mpingo uyenela kugwapo posamalila okalamba ? Boazi atadziŵa kuti anacita kupempha kuti akunkheko , anamulola kukunkha ngakhale pa mitolo ya tiligu . — Ŵelengani Rute 2 : 5 - 7 , 15 , 16 . Ana anu ayenela kusankha okha kukhala paubale ndi Yehova . Petulo anawauza kuti “ mapeto a zinthu zonse ayandikila ” . CAKA ciliconse , maphunzilo a Baibo masauzande ambili amadzipeleka kwa Yehova na kubatizika . Ngati mwana wanu satsatila malamulo anu , musalephele kum’patsa cilango . Mtumwi Paulo analangiza Akhristu anzake kuti : “ Landilanani , monga mmene Khristu anatilandilila . ” PA September 6 , 1926 , woyang’anila woyendela wina anabwelela kwao ku Japan monga mmishonale kucokela ku United States . 32 : 1 . ( Mat . 14 : 31 ; 2 Ates . Zinthu monga mafilimu , maseŵela a pa kompyuta , na zosangalatsa zina , zimalengetsa anthu kuona ngati zamizimu n’zokondweletsa . ( Eks . 23 : 24 , 25 ) N’zomvetsa cisoni kuti Aisiraeli ambili sanamvele malangizo a Mulungu . Pambuyo pa zaka 100 , magazini ina ya Nsanja ya Mlonda inakamba kuti mizinda yothaŵilako inali kuimila “ makonzedwe a Mulungu otiteteza kuti tisafe cifukwa cophwanya lamulo lake lokhudza kupatulika kwa magazi . ” Ngati zimene munthu alakalaka sizicitika , zingam’dwalitsa mtima . Gulu la Mboni za Yehova linadzipeleka kukathandiza anthu pambuyo pakuti cimphepo camkuntho cawononga m’delali . 4 : 17 ) Yesu anaphunzitsa ophunzila ake kugwila nchito imeneyi . ( Yobu 42 : 1 , 2 ) Ndipo zimenezo n’zimenedi zinacitika . 4 : 25 ) Pamene mapeto a dzikoli akuyandikila , tifunika kucita zinthu mogwilizana kwambili kuposa ndi kale lonse . Mulungu wamphamvu zonse ndi yekhayo woyenela kulamulila . N’cifukwa ciani Mulungu walola kuti zimenezi zindicitikile ? ” Ndili mu mtengowo ndinaona nyumba yathu ndi katundu wathu zikuonongedwa . Komabe anandicitila cifundo cifukwa ndinali wosadziŵa ndi wopanda cikhulupililo . ” ( 1 Tim . Acicepele anayi othaŵa kwawo atafika mumpingo wina , akulu osiyana - siyana anawaphunzitsa kuyendetsa motoka , kutaipa , kulemba makalata ofunsila nchito , ndi kugaŵa bwino nthawi kuti azitumikila Yehova mokwanila . ( Agal . 1 : 22 ; 1 Yoh . 4 : 21 . Cifukwa copewa kudzipatula kwa Yehova na gulu lake , iwo amapeza nzelu zopindulitsa na kuzigwilitsila nchito kuthandiza banja lawo . 46 : 31 - 34 ) Ngakhale n’conco , io analola Aisiraeli kukhala m’dzikolo . Pamapeto pake , tidzakambilana zinthu zina zimene tingacite kuti tikulitse khalidwe lodziletsa . N’cifukwa ciani tifunika kuphunzila kukonda malamulo a Mulungu ? Akulu amasamalila maudindo ambili ofunika amene ngati sangawasamalile mwamsanga mpingo ungakhale pangozi . Mbadwa za Yakobo zinakhala mu Iguputo zaka zoposa 200 , m’cigawo cochedwa Goseni pafupi ndi mtsinje wa Nailo . YELEKEZELANI kuti ndinu Mkristu m’nthawi ya atumwi . Ganizilani phunzilo limene mwatengapo pa zimene mwaŵelenga Kwa Yehova na Yesu , nkhani ya kukhululukilana ndi yaikulu kwambili . ( Mat . 24 : 45 - 47 ) Ndikayang’ana kumbuyo zaka 50 zimene ndakhala mu utumiki wa nthawi zonse ndimakondwa , ndipo ndimayamikila kwambili kuti Yehova wadalitsa ubale wathu wa padziko lonse . Mwadala io amafalitsa mabodza n’colinga cofuna kulepheletsa anthu kudziŵa Atate , Yehova Mulungu , ndi Mwana Wake , Yesu Kristu . ( Ŵelengani Deuteronomo 6 : 6 , 7 . ) 11 : 26 ) Ifenso tikamaganizila mmene malonjezo a Yehova adzakwanilitsidwila , cikhulupililo ndi cikondi cathu pa Mulungu zimalimba . ( Yoswa 11 : 20 ) Adaniwo anagonjetsedwa cifukwa analephela kuvomeleza kuti Yehova anali kumenyela nkhondo anthu ake . ZIMENE CINALI KUIMILA M’kupita kwa nthawi , amai ndi abale anga 6 anabatizidwa . Kodi mungaleke kusonkhana kapena mungasiye Yehova ndi gulu lake ? Asa , Yehosafati , Hezekiya , Yosiya TSAMBA 21 Ndipo buku yakuti Watch Tower Publications Index ili na kamutu kakuti “ Beliefs Clarified . ” ( Kamvedwe Katsopano ka Ziphunzitso ) Pamenepo pali m’ndandanda wa kamvedwe katsopano ka Malemba kuyambila mu 1870 . Iye anati : “ Anthu a m’dziko la Satanali amalimbikitsa acicepele kucita maphunzilo apamwamba , kukhala ochuka , ndi kukhala na cuma coculuka , ndipo amati zimenezi ndiye zolinga zabwino . ( Gen . 1 : 1 ) Ise anthu timadziŵako zocepa cabe pa zinthu zambili zimene Mulungu anapanga , monga thambo , kuwala , ndi mphamvu yokoka zinthu kuti zigwe pansi . Ndithudi , tsoka kwa ine ngati sindilengeza uthenga wabwino ! ” Yakobo anayelekezela umoyo wathu ndi wa mlimi . TSAMBA 23 • NYIMBO : 111 , 109 Munali ndalama zambili . Kodi ningayembekezele Yehova moleza mtima kapena ningayese kuthetsa vutolo panekha ? ’ — Miy . 11 : 2 ; ŵelengani Mika 7 : 7 . Koma Atate wake , Yehova , “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , ” amathandizabe anthu amene afunika thandizo . Zimenezi zinanicititsa cidwi . Abale a kumeneko anakondwela kwambili kuona M’bale Franz atavala covala ca Cifilipino cochedwa barong Tagalog pokamba nkhani . ( Aroma 1 : 25 ) Ngati timvetsela zimene iwo amakamba , pang’ono ndi pang’ono tingacoke kwa Yehova , ndipo cikondi cathu pa iye cingayambe kuzilala . — Aheb . Tiyeni tigwilitsile nchito Baibulo langa . Ganizilani za umoyo wake , zolinga zake , na zofooka zake . Ndipo utumiki umenewu walimbitsa banja lathu . ” Kodi Petulo anacita ciani atayamba kumila ? Timasangalala kwambili kuona banja limeneli likupita patsogolo . Ndipo mwana wao wamkulu wamwamuna anayamba upainiya . ” Baibo imaonetsa kuti atumiki ena akale okhulupilika a Mulungu , nthawi zambili anali kuona kuti sakanakwanitsa kupilila mavuto awo . ( 1 Maf . Pa tsiku laciŵili la makambilano athu usiku , M’bale Albu anacondelela akulu anai aja kuti agwilizane nafe . N’ciani cingakulimbikitseni ngati mumaopa kuceleza alendo ? Bungwe la akulu ndi lofunitsitsa kupeleka uphungu ndi cilimbikitso kwa m’baleyo , koma zili kwa iye kukwanilitsa ziyeneletso za m’Malemba . ( b ) Kodi “ nkhosa zina ” ziyenela kucitanji pothandiza “ Isiraeli wa Mulungu ” ? Ndipo zili ndi ciyembekezo cotani ? A Zulu : Baibulo ndi limene limatithandizanso kudziŵa utali weniweni wa nthawi zokwanila 7 . Cofunika kwambili ndi kukhala na makhalidwe abwino acikhristu amene adzakuthandizani kucita zambili potumikila Yehova . Beck anati : “ Malinga n’zimene Ayuda amakhulupilila , Aisiraeli opanduka anamutsutsa Mose na kukamba kuti : ‘ Mose wamenya thanthwe ili cifukwa adziŵa kuti n’lofooka . Pamene Yosefe anali ndi zaka 17 , tsiku liina anapita kukathandiza abale ake kugwila nchito yaubusa ndipo anaona zoipa zimene io anali kucita . Tsopano nimalengeza uthenga wamtendele wa m’Baibulo kwa aliyense amene angamvetsele . Cocitika Cimene Simuyenela Kuphonya 26 Pambuyo pake , Samueli ndi Sauli ananyamuka kupita ku nyumba ya mneneliyo ndipo m’njila anali kuceza . Ganizilani mmene anaonetsela kulimba mtima patsiku lomaliza la moyo wake padziko lapansi . Mwina zingaoneke kuti njila yapafupi ni kum’funsa zosoŵa zake kapena zimene afuna . Ndipo tikakumana nawo mu ulaliki , kwa nthawi yoyamba mu umoyo wawo , angafune kumvetsela uthenga wathu wopatsa ciyembekezo . Kazuhiro anapemphela na mtima wonse kwa Yehova . Kodi mutumikila kosoŵa kapena monga mmishonale kudziko lina ? Kapena kodi mwayamba kusonkhana mumpingo wa cinenelo cina ? Mtumwi Paulo anafotokoza kuti Akristuwo anali ogwilizana ngakhale kuti anali ndi maluso ndiponso mautumiki osiyanasiyana . Komiti ya Ogwilizanitsa Komabe , pa Salimo 37 : 29 Baibo imati : “ Olungama adzalandila dziko lapansi , ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya . ” Pa tsiku loyamba lokumbukila cikwati cathu , kunyumba kwathu kunabwela mnyamata wa Mboni . “ Azipempha ndi cikhulupililo , osakayikila m’pang’ono pomwe . ” — YAK . ( 2 Ates . 1 : 9 ) Ndiyeno , tingaŵelenge naye lemba la Genesis 2 : 16 , 17 , limene limaonetsa kuti cilango caucimo ndi imfa . Anthu ena akathaŵa kwawo , amakakhala m’dela lina m’dziko lawo lomwelo . Koma ambili amathaŵila kudziko lina , kumene umoyo umakhala wosiyana ngako na umene anajaila . 13 Mbili Yanga Kupilila Ziyeso Kumabweletsa Madalitso Komabe , cifukwa ca cikondi cake cacikulu , Mulungu anapeleka zimene tinali kufunikila kuti timasuke . Ndinali kuti ndikachula dzina lakuti Yehova mwamuna wanga anali kukwiya kosaneneka . ” Conco , Yehova wanipatsa mwana mwamuna , mpongozi , na adzukulu atatu . ” — 3 Yoh . 4 . Pa funso imene tikukambilana , katswili wina anati n’zokaikitsa ngati Isaki ndi Abulahamu ananyamula “ lawi la moto ndi kulisunga loyakabe paulendo wawo wonse . ” 11 : 45 . Malinga ndi Miyambo 14 : 35 , kodi tiyenela kucita ciani ? Yesu anati : “ Pitilizani kufunafuna ufumu coyamba ndi cilungamo cake , ndipo zina zonsezi zidzaonjezedwa kwa inu . ” [ 1 ] ( ndime 3 ) Malinga ndi lemba la Salimo 87 : 5 , 6 , n’kutheka kuti m’dziko latsopano , Mulungu adzaulula maina a anthu onse amene adzakhala akulamulila ndi Yesu kumwamba . — Aroma 8 : 19 . ( Nyimbo 8 : 8 - 10 ) Mofananamo , Akristu amene ali pa cisumbali ayenela kukhala okhulupilika kwa wina ndi mnzake . 7 : 46 ) Cikondi cotelo cingathandizenso makolo kuwafika pamtima ana awo . Koma ndi zozikidwa pa Malemba , omwe ndi coonadi . — Yes . Anatenga mankhwala na zina zothandizila munthu akavulala , ndipo anatsuka cilondaco ndi mankhwala n’kumangapo na bandeji . Iwo anathandiza anthu ena kumvetsetsa coonadi pogwilitsila nchito magazini a Zion’s Watch Tower ndi zofalitsa zina . Ngati tiuza ena za nkhaniyo kukali nthawi , zingabweletse mavuto osaneneka . Inoki ayenela kuti anali pafupi kuphedwa mwankhanza na adani ake pamene Yehova anamusamutsa Kodi tiyenela kucita ciani tikakumana na mavuto aakulu mu umoyo ? 7 : 2 , 9 , 36 ; 1 Tim . 4 : 1 - 3 ) Apa satanthauza kuti wacinyamata kapena wacitsikana akayamba kutenthedwa na cilakolako basi akwatile , yayi . Mzimu woyela si munthu . Masiku ano , nafenso tiyenela kumvela Mau a Yehova osati mabodza a Satana . Kusintha maganizo kungakhale kofunika pankhani yokhudza zolinga zakuuzimu . Tikupemphani kuti mukakhale nafe poyamikila mphatso yaikulu ya Mulungu imeneyi . Idzafotokozanso cifukwa cake na ise tifunika kukhala ofunitsitsa kutamanda Mulungu wathu . Anafunika kupeleka nsembe , kusamba thupi lonse , kapena kuthilidwa madzi . — Lev . , caputala 11 mpaka 15 ; Num . , caputala 19 . Ŵelengani Yesaya 40 : 30 . Ngati mumakhulupilila Mulungu , kodi mumaona kuti pemphelo limakuthandizani paumoyo wanu ? N’zoonekelatu kuti ofalitsa m’dzikoli amakwanitsa kulalikila anthu ocepa cabe . ( Gen . 22 : 18 ; 26 : 4 ; 28 : 14 ) Mbadwa zao zinali kudzaculuka ndi kudzakhala m’dziko limene Mulungu analonjeza . ( Gen . Iye anati : “ Inu munamva kuti anati , ‘ Uzikonda mnzako ndi kudana ndi mdani wako . ’ ( Machitidwe 5 : 18 - 20 ; 12 : 6 - 11 ) Posacedwapa m’dziko lina la mu Africa munali nkhondo yoopsa . Iye anakamba kuti anali kudzimva conco cifukwa ca kupanda ungwilo . Ndi maganizo ati amene tiyenela kupewa ? Nanga n’cifukwa ciani ? Nditangowauza zimenezi , anakhumudwa kwambili . Makadi a ulaliki anathandiza ofalitsa onse kulalikila uthenga momveka bwino . Amati miyala ina ya kacisi inali kufika mamita 11 muutali mwake , mamita 5 muufupi , na mamita atatu kukwela m’mwamba ! M’nthawi ya Nowa , angelo ena osadziŵika ciŵelengelo , “ anasiya malo awo okhala ” m’banja la Mulungu kumwamba . ( a ) Kodi Yesu anayankha bwanji pempho la atumwi ake ? M’dziko latsopano , tidzapindula mokwanila ndi paradaiso wauzimu . ( 1 Petulo 2 : 9 ) Yehova adzadalitsa anthu onse omvela kudzela mu Ufumu wake umenewu . Pakakhala vuto limene lingakhudze banja lawo na tsogolo lawo , anali kuuza mwamuna wake moona mtima . N’cifukwa ciani iye sanakayikile kuti zimenezi zidzacitikadi ? Popeza munapeleka moyo wanu kwa Yehova , tsopano mungakambe mwacidalilo kuti : “ Yehova ali kumbali yanga , sindidzaopa . Popeza kuti anthu ambili ali na cikondi cadyela , dzikoli lakhala ‘ lovuta . ’ Baibo imafotokoza momveka bwino masomphenya a mahosi anayi amphamvu ndi okwelapo ake cakuti tikamaŵelenga , timakhala ngati tikuwaona m’maganizo mwathu . Ikani Mtima Wanu pa Cuma Cauzimu , June Sititenga mbali pa zocitika za m’dzikoli : Sititenga mbali m’zandale kapena m’nkhondo cifukwa cakuti ndife okhulupilika ku Ufumu wa Mulungu Popeza kuti tonse ndise opanda ungwilo ndipo timacimwa , timadziŵa kuti wina mumpingo akhoza kutilakwila kapena ise tingalakwile ena . ( 1 Yoh . Ndinazindikila kuti ndifunika kusintha umoyo wanga kothelatu . Popeza Yesu anakhala Mfumu mu 1914 , n’cifukwa ciani zinthu padzikoli zikuipila - ipila ? 1 , 2 . ( a ) Kodi ndi cikwati ca ndani cimene cidzabweletsa cisangalalo coculuka kumwamba ? Onetsani cikhulupililo mwa kuuzako ena uthenga wabwino mpata ukapezeka ( Onani ndime 12 ) Rakele sanali kubeleka kwa nthawi yaitali , koma pomaliza pake anabala Yosefe amene Yakobo anamuona kuti anali mwana wapadela kwambili popeza anali atabadwa iye atakalamba . Johannes Rauthe ali mu ulaliki , mwina ca m’ma 1920 Mwacitsanzo , iye anakamba kuti odala ndi anthu amene ali ndi njala ndi ludzu . Mwacitsanzo , Mulungu analonjeza kuti adzaononga dziko la Satana . Mau a Mulungu amati : “ Dziko likupita limodzi ndi cilakolako cake , koma wocita cifunilo ca Mulungu adzakhala kosatha . ” ( 1 Yoh . Munthu woyamba amene ndimakonda kwambili ndi mkazi wanga , Susan . Nthawi ina ndinapemphela kuti : “ Mulungu , ndinakupemphani kuti muwacilitse atate . ( Deuteronomo 19 : 18 , 19 ) Conco ngati munthu wanama bodza m’khoti n’colinga coti atenge colowa ca wina , anali kumulipilitsa . Don anacita zinthu moleza mtima kwa zaka zoposa 14 , kuti athandize munthu wosoŵa kokhala ameneyu . Palinso makonzedwe oti Baibulo lokonzedwanso liyambe kupezeka m’zinenelo zinanso . Koma m’kupita kwa nthawi , iye anapandukila Mulungu na kupha m’bale wake . CIKHULUPILILO Zimene anacitazi zinabweletsa mwayi ‘ woteteza ndi kukhazikitsa mwalamulo nchito ya uthenga wabwino . ’ ( Afil . PA NTHAWI ina , Akristu ena acinyamata anaganiza zopita kukapenyelela vidiyo ku malo oonetsela mavidiyo . Iwo ananiphunzitsa zambili . 7 : 14 - 17 . Malo a Akazi m’Kakonzedwe ka Yehova , 8 / 15 Mwacitsanzo , pamene Adamu na Hava anaphwanya lamulo la Yehova , anathaŵa n’kukabisala . ( b ) Ndi malangizo ati amene anathandiza abale a ku Kolose kukhalabe olimba ? Kukhumudwitsana , kusamvetsetsana , ndi kusalankhulana bwino , kungabweletse mavuto ngakhale m’mabanja ogwilizana kwambili . ( Mat . 11 : 29 ) Nthawi zonse anali kuleza mtima ndi ophunzila ake mosasamala kanthu za zofooka zao . Koma abale kumeneko anali kuona zinthu mosiyanako . 15 : 13 ) Tikamadalila Mulungu ndi kutsatila mapazi a Mwana wake , timakhala olimba mtima . — Sal . Mosiyana na iwo , Yesu sanali kudzisiyanitsa na gulu la anthu , cakuti nthawi zina anthu sanali kumuzindikila . ( Salimo 65 : 2 ) Mulungu amatikonda kwambili ndipo amatisamalila , cakuti zinapangitsa mtumwi Yohane kulemba kuti : “ Mulungu ndiye cikondi . ” — 1 Yohane 4 : 8 . Ngati Baibulo si buku locokela kwa Mulungu , kodi Mulungu akanaiteteza kuti anthu asaiwononge ? 39 : 12 . Kodi inunso mumamvela monga mmene Crystal anamvelela ataŵelenga za amuna anayi okwela pa mahosi a m’buku la Chivumbulutso ? Kuyambila cakumapeto kwa m’ma 1800 , ni udindo wofunika uti umene M’bale Russell anali nawo ? Conco , Yehova amafuna kuti mukhale na zolinga zimene zidzakupatsani mwayi woonetsa kuti mumakonda iye ndi anthu anzanu . — Ŵelengani Mateyu 22 : 36 - 39 . CAPAKATI PA MZINDA WA ROMA KU ITALY , PALI CIPILALA CIMENE CIMACITITSA CIDWI ALENDO OCOKELA KOSIYANA - SIYANA OKAONA MALO . Mwacitsanzo , ngati tipewa ‘ kudzionetsela ndi zimene tili nazo pa moyo wathu , ’ ndipo m’dela lathu timadziŵika monga Mboni ya Yehova yokonda mtendele , tingapewe kuvutitsidwa ndi anthu acifwamba . — 1 Yoh . 2 : 16 ; Miy . OLOŴETSEDWAMO : Yehova ndi Davide N’ciani cimene Kaini anacita atapatsidwa mwayi wokhala kumbali ya Yehova ? ( Life in Biblical Israel ) Nkhalango zimenezi zinali ndi mitengo ikuluikulu ya paini , oki ndi telebeti . 16 : 35 - 40 ) Pamene cigulu ca anthu aukali cinafuna kuvulaza Akristu ena ku Efeso , ndipo woyang’anila mzinda atakhalitsa cete anthuwo , iye anawakumbutsa zimene malamulo a Roma amanena . ( Mac . Khalani bwenzi , osati cabe mphunzitsi . Muzicita maseŵela olimbitsa thupi kaŵili - kaŵili . 11 : 9 - 13 . Ndinaphunzilanso kumudalila osati kudzidalila kapena kudalila anthu ena . ( Mac . 17 : 22 , 23 ) Anali kusintha - sintha ulaliki wake kuti ugwilizane ndi anthu amene anali kuwalalikila , n’colinga cakuti ‘ mulimonse mmene zikanakhalila apulumutseko ena . ’ — 1 Akor . ( Maliko 7 : 7 ; Akolose 2 : 8 ) Conco , iye anaona kuti tsopano ni nthawi yakuti uthenga wabwino “ ulalikidwe moyenelela padziko lonse kuti anthu asanamizidwe na ziphunzitso zacilendo za anthu . ” Mlongo wina wokhulupilika anati : “ Ukauzako anthu za madalitso a Ufumu wa Mulungu , umazindikila kuti anthuwo alibiletu ciyembekezo ciliconse . Ndipo amaona mavuto awo kuti sadzatha . ” Kuti munthu akhale pa ubwenzi wolimba na Yehova , amafunika kucita zinthu ziŵili — kumvetsela kwa iye , ndiponso kukamba naye . Kuyambila zaka za m’ma 400 B.C.E . , panali Ayuda amene anali kukhala m’zigawo 127 mu Ufumu wa Perisiya . Mofanana ndi Mose , sitimaona kuti zaka zimene tatumikila Yehova ndi kutaya nthawi . Ni makhalidwe ati amene anacititsa kuti ophunzila a Khristu asakhale ogwilizana ? Nanga tidzakambilana mafunso yati ? Kodi mungaikonde mphatso yotelo ? Mwina pa phwandolo panabwela anthu ambili kuposa amene anali kuyembekezela . Ganizilani za kufunika kopezeka pa Cikumbutso . Tsiku lina Yesu anapita kukalalikila ku Galileya . Iye anati : “ Sindinali kuikonda nchito yolalikila . Lipoti linanso linati : “ Caka ciliconse , anthu amene amafa ndi njala ni ambili kuposa amene amafa ndi matenda a AIDS , maleliya , na TB tikawaphatikiza pamodzi . ” Kodi muyenela kukhala na colinga cotani ? Kodi n’zoona kuti Yehova anali wokhumudwa na atumiki ake cifukwa cobwelela m’mbuyo panchito yolalikila , mkati mwa nkhondo yoyamba ya dziko lonse ? Kenako Mose ananyamuka n’kupita kwa Datani ndi Abiramu , ndipo akulu a Isiraeli anapita naye limodzi . Monga kholo muli ndi udindo wopeleka malamulo kwa ana anu . Conco , Mulungu sangagwilitsile nchito Satana kuzunza anthu amene iye Mdyelekezi amawasonkhezela kucita zoipa . ONANI ZINTHU MOYENELA Kucita zimenezi kumabweletsa mapindu ambili . 6 , 7 . ( a ) N’ciani cimaonetsa kuti Yehova amawasamalila atumiki ake onse ? Nanga ena 9 ali kuti ? ” Ndidzamutamanda ndi pakamwa panga mosalekeza . Ndidzadzitamandila mwa Yehova . Tsopano , tiyeni tikambilane zimene amuna aŵili okhulupilika akale anacita kuti ‘ akondweletse Mulungu . ’ — Aheb . Atangokumana koyamba , anayamba kukambilana zokhudza mabanja awo . ( Tito 2 : 14 ) Ndiponso , timayamikila citsanzo ca Akristu odzozedwa okhulupilika , amene anatsogolela panthawi zovuta , ndi kutumikila monga mboni ziŵili zophiphilitsa . Iye yekha ndiye ‘ amatiphunzitsa kuti zinthu zitiyendele bwino , amene amaticititsa kuti tiyende m’njila imene tiyenela kuyendamo . ’ Yehova anadziŵa kuti anthu ake afunikila cilimbikitso . Mwacitsanzo , kholo lina linatilembela mau pa kapepa kutidziŵitsa kuti mwana wathu wina anali kukamba mau oipa m’Nyumba ya Ufumu . Koma monga atumiki a Mulungu , anapeza cimwemwe ceni - ceni cifukwa cokhala okhulupilika kwathunthu kwa iye . ( Danieli 2 : 44 ) Ufumu wa Mulungu ndi boma leni - leni . Mu 2012 , Perrine analimba mtima , ndipo iye na mwamuna wake Louis anakukila ku Madagascar . Pamene Yesu anauza ophunzila ake kuti “ lekani kudela nkhawa moyo wanu , ” anali kutanthauza kuti ayenela “ kuleka kudandaula . ” Tingacite ciani kuti cikumbumtima cathu cizititsogolela bwino ? Yosefe atafotokoza loto laciŵili kwa atate ake ndiponso kwa abale ake , iwo sanayankhe bwino . 4 : 34 ; 17 : 4 ) Mofananamo , nchito imene tapatsidwa masiku ano imalemekeza Yehova . “ Padziko lapansi padzakhala tiligu wambili . Pamwamba pa mapili padzakhala tiligu woculuka . ” — Salimo 72 : 16 . N’ciani cionetsa kuti ciyamikilo na cilimbikitso zimathandiza popeleka uphungu ? Monga Mkhristu wobatizika , ubwenzi wanu na Yehova si uli ngati cuma ca banja cimene mungalandile monga coloŵa . 27 Pindulani Mokwanila ndi Cakudya Cakuuzimu Cimene Yehova Amapeleka Conco , mu June 1940 atakwanitsa zaka 17 , anachova njinga pa msenga wa makilomita 105 kupita ku tauni ya Scarborough kukatumikila monga mpainiya . Komanso , izi zinacititsa kuti Yehova adziŵike m’madela onse a Ufumu wa Mediya ndi Peresiya , ngakhale ku madela akutali kwambili . — Dan . Ndili ndi banja lakuuzimu labwino kwambili . ” Akulu sangakusankhileni zocita , koma angakuthandizeni kuti mupange zosankha zimene zidzakusangalatsani m’kupita kwa nthawi . — 2 Akor . ( Luka 20 : 47 ) Iye anali wosauka kwambili cakuti copeleka cake cinali cofanana ndi malipilo a munthu amene waseŵenza mphindi zocepa . Kuwonjezela apo , moni wacikondi umenewo unalimbikitsa Akhristu ena na kuwathandiza kukhalabe olimba m’cikhulupililo . Moŵa utatha m’mutu , ndinayamba kudziimba mlandu . Ndithudi , Yehova anali kutsogolela anthu ake . Kodi mmene Boazi anacitila zinthu ndi Rute , anaonetsa bwanji mmene Yehova amaonela alendo ? Koma ndi anamwali anzelu okha amene anakhalabe maso . Baibulo lonse kapena mbali yake , lipezeka m’zinenelo zoposa 2,800 . Timadzipeleka kwa Yehova Yekha ngati tilambila iye yekha ndi kumuika patsogolo mu umoyo wathu . Komanso tonse timatsatila malangizo a Yehova m’malo moti aliyense azicita zimene aona kuti ndiye zabwino . Komanso , ana athu anali kukonda kusunga Malemba pa mtima . Iye anacititsa Adamu na Hava kupandukila Mulungu . Onani zimene Mose anauza anthuwo . Iye anati : “ Kodi ticite kukutulutsilani madzi m’thanthweli ? ” Cimene anali kudziŵa n’cakuti adzamwalila na kupumula . ( Chiv . 22 : 17 ) Zoonadi , a “ nkhosa zina ” anamva pamene Akristu odzozedwa ananena kuti “ Bwela ” ndipo ionso agwilizana ndi gulu la mkwatibwi mwa kunena kuti “ Bwela ” kwa anthu onse okhala padziko lapansi . — Yoh . Kuti mudziŵe kumene miyambo yambili ya pa Khrisimasi inacokela , onani nkhani yakuti “ Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi . . . Ngakhale n’conco , muyenela kuona zinthu mmene Yehova amazionela . Daniel anati : “ Ndinapitilizabe kutumila mtsikanayo mameseji ngakhale pamene ndinakhala mpainiya . ” Kodi mumaika kwambili maganizo anu pa mavuto a m’dzikoli kapena pa Ufumu wa Mulungu ? Caka ciliconse Cikumbutso cimakhala capadela kwambili kwa ife . Pambuyo pake , tinayamba kulembelana makalata , ndipo mu 1956 , tinakwatilana . Miseu yabwino inali yofunika kuti asilikali aziyenda mofulumila , ndipo Aroma anali akatswili popanga miseu imeneyo . Kungakhale kupanda nzelu ndiponso kulakwa kusiya Yehova ndi anthu ake cifukwa cakuti munthu winawake mumpingo watilakwila kapena wakamba mau oipa . Yehova sasintha , ndipo ndi wodalilika . Baibo imakamba kuti tifunika kupitiliza ‘ kukhala atsopano mu mphamvu yoyendetsa maganizo athu . ’ ( Aef . Koma zaka zimenezi zikalibe kufika , ca m’ma 700 B.C.E , wolemba Baibo Yesaya analemba kuti : ‘ Dziko lapansi ni lozungulila . ’ — Yesaya 40 : 22 . Nthawi zambili ndinali kutsala pang’ono kufa cifukwa ca kuledzela . ( 1 Tim . 4 : 15 , 16 ) Conco , Akhristu amene ali na udindo wa m’malemba wopeleka cilango cauphungu kwa ena , ayenela kupitiliza kumvela malamulo a Yehova na mtima wonse . “ Kristu anavutika cifukwa ca inu , ndipo anakusiyilani citsanzo kuti mutsatile mapazi ake mosamala kwambili . ” — 1 PET . 8 : 9 - 18 ) Mofananamo , ifenso timapindula ndi misonkhano yampingo , yadela ndi yacigawo . Ndipo zozizwitsa zimenezo zimapeleka cithunzi ca zinthu zabwino zimene zidzacitika padziko lonse mtsogolo . Adamu anaphwanya lamulo la Mulungu mwadala . Zimene anacitazi ni chimo . Iye anati : “ Tapambana milandu kukhoti cifukwa ca kulimba mtima kwanu . Iye anapempha Yehova kuti atsegule njila yakuti alalikile . N’cifukwa ciani Yesu anakamba kuti sitingatalikitse moyo wathu pang’ono mwa kuda nkhawa ? ( Yohane 4 : 23 ) Kwa zaka zambili , Ayuda anali kuona kuti kacisi wa ku Yerusalemu anali likulu la kulambila kwao . ( Yoh . 3 : 16 ; 1 Tim . 2 : 3 , 4 ) Kulemekeza maganizo a anthu ena kudzatithandiza kusunga mgwilizano wathu wacikristu . Akaidi pafupifupi 40 tinali kugona mu kanyumba katenti kamene kanakonzedwa kuti muzigona anthu 10 cabe . 15 : 11 , 14 ) Ifenso , tiyenela kutumikila Mulungu ndi mtima wathunthu kuti tikhale paubale wolimba ndi iye , tsopano ndi mtsogolo . Baibulo landiphunzitsa kulemekeza anthu onse , amuna ndi akazi omwe . Landiphunzitsanso kudziona moyenela . Timalakalaka kugwilitsila nchito anthu amenewa pa nkhani za ndale , koma sizingatheke . . . . NYIMBO : 39 , 30 Cofunika kwambili ndi kutumikila Yehova mokhulupilika . — 1 Akor . Conco , m’pake kuti Baibo pokamba za umunthu watsopano , imatsiliza na mfundo yamphamvu iyi : “ Kuwonjezela pa zonsezi , valani cikondi , pakuti cimagwilizanitsa anthu mwamphamvu kwambili kuposa cinthu cina ciliconse . ” — Akol . ( Aroma 1 : 20 ) Mwa ici , Nowa anakhala na cikhulupililo colimba mwa Mulungu . Koma Baibulo limanena momveka bwino kuti “ cizindikilo ca Mwana wa munthu ” cidzaonekela kumwamba ndipo Yesu adzabwela “ pamitambo ya kumwamba . ” ( Mat . Imatilimbikitsa ( 1 ) kutengela citsanzo ca Yesu mosamala kwambili , ( 2 ) kukonda abale athu ndiponso ( 3 ) kukhululukila ena mocokela pansi pa mtima . Kodi tidzakambitsilana mfundo ziti zimene zingatithandize kukulitsa cikondi cathu pa Atate wathu wakumwamba , Yehova ? Pofika mu 1931 ciŵelengelo ca anthu a ku Poland m’dziko la France cinali 507,800 , ndipo ambili anakakhala kumalo amigodi kumpoto kwa dzikoli . Akadzaukitsidwa , adzasangalala kwambili kudziŵa za kutulutsidwa kwa Baibulo m’Cituvalu . Muziwauza ana anu kuti mumawakonda , ndipo zocita zanu zizionetsa kuti mumawaona kukhala ofunika kwambili . PAMENE ciphadzuŵayo — mkwatibwi — acitoŵala kwa mkwati wake pa tsiku la cikwati , nayenso mwamuna atakongola mocititsa kaso , cimwemwe cawo cimakhala cosaneneka . 2 : 6 ) Nanga Paulo anali kukamba ciani pamene analemba za “ maziko olimba a Mulungu ” ? Nanga n’cifukwa ciani nafenso ndife otsimikiza ? Mukapita nao muutumiki , apatseni zocita kuti azidzimva kukhala ofunika . * Iye anakamba kuti : “ Ngati kuti kunalibe njila zimenezi , sinidziŵa kuti nikanacita bwanji kuti nikhalebe olimba kuuzimu . ” Kuonjezela apo , ena amagwilitsila nchito udindo wao kuti acite zinthu zokondela anzao kapena abale ao . Ndipo Yehova nayenso amakunyadilani ! Patapita cabe masiku 5 , ofesiyo inawayankha kuti , “ Bwelani , tifuna apainiya ambili kuno ! ” ( Afilipi 4 : 13 ) Paulo analimbikitsidwa na mzimu woyela wa Mulungu . 2 : 11 ) Conco , cifukwa cosakhala mbali ya dziko sitiloŵelela m’mikangano ya dziko . — Ŵelengani Yohane 15 : 18 , 19 . Onani kuti ulosiwu wanena kuti Ufumu umenewu adzalamulila “ anthu a mitundu yosiyanasiyana ndi olankhula zinenelo zosiyanasiyana . ” POSACEDWAPA , wofufuza wina anafunsa acinyamata oposa 800 ocokela m’zipembedzo 12 zosiyanasiyana , kuti akambe ngati amakhulupilila kuti Yesu amayankha mapemphelo . Iye anali wodziŵa kulankhula , anali kucilitsa odwala , komanso anakwanitsa ngakhale kupatsa cakudya anthu amene anali na njala . Conco nimacita zimene ningakwanitse kuti nithandize ena . Ngakhale kuti ndinu wacicepele kapena muli ndi thanzi labwino , mungaziona kuti zocita zanu mu utumiki ndi zocepa poyelekezela ndi za anthu ena a Mulungu . Anthu ambili mumpingo akukumana ndi mavuto aakulu . Komanso , Yesu akanakamba kuti Ayuda afunika kupeleka msonkhowo , ndiye kuti ophunzila ake sembe anayamba kumuzonda . 31 Akristu ayenela kutsimikiza kuti cithandizo ciliconse cimene angalandile sicikuphwanya mfundo za m’Baibulo . ( Ŵelengani Aroma 5 : 12 ; 6 : 23 . ) ( 2 Timoteyo 3 : 16 ) Uthenga wake ungatithandize ngako pa umoyo wathu . Kenako m’fanizo la anamwali 10 , Yesu anakamba kuti anamwali asanu anali opusa . Pochula mfundo imeneyi , Yesu sanali kutanthauza kuti hafu ya odzozedwa adzakhala opusa . 27 : 14 ) Cikondi codzimana cimaticititsa kukhala wolimba mtima ngakhale moyo wathu utakhala pangozi . ( Yoh . 12 : 3 ) N’zovuta kuti anthu opanda ungwilo akhale odzicepetsa . ( Mateyu 5 : 23 , 24 ) Conco , muyenela kukambilana ndi m’bale wanu . Komanso , mutu wa nyimbo wakuti “ Tetezani Mtima Wanu , ” unasinthiwa n’kukhala , “ Titeteze Mitima Yathu . ” Ngati mufunitsitsa kutumikila Yehova , gwilitsilani nchito mwai umene iye wakupatsani pamene mukali wacinyamata . Mlongo wina wa mumpingo mwawo , amene ni mpainiya anayamba kucita nawo ulaliki umenewu . Nthawi ina ndinalibe fodya ndipo ndinavutika kwambili . Ndinatenga fodya amene anatsalila pa kambale koikapo phulusa la ndudu , ndi kupanga ndudu ya fodya pa kapepala . ( Yoh . 5 : 28 , 29 ) Koma Satana alibe tsogolo labwino . Aisiraeli anakhala mboni za Yehova m’njila ziti ? Izi zinali zosiyana kwambili ndi atsogoleli ankhanza ndi odzikonda a mitundu ina . Gwen : Ndinabadwa m’caka ca 1944 ku London . Ngakhale kuti Paulo anali na umoyo mofanana ndi anthu onse , kodi n’ciani cimene anaika patsogolo maka - maka ? Mofanana ndi zimenezi , kukonda zosangulutsa kungatifooketse mwauzimu . Koma mau akuti “ paladaiso wauzimu ” ndi akuti “ kacisi wauzimu ” satanthauza zinthu zofanana . Mofanana ndi anthu ambili amene ndi atsopano m’cikwati , zinali kuwavuta kuti azigwilizana cifukwa ca kusiyana umunthu . 19 : 17 , 18 . Makolo ena amaona kuti ana akafika zaka za m’ma 13 mpaka 19 , zimavuta kukambilana nao . Iwo akafika zaka zimenezi safuna kukambilana maganizo ao ndi zimene amafuna . Mulungu anatuma Haneni kuti akam’dzudzule cifukwa cosadalila Yehova . Zakeyu anati : “ Ambuye , ine ndipeleka ndithu hafu ya cuma canga kwa osauka . N’cifukwa ciani zifunika kuonekela bwino kwa ena kuti ndise odzipatulila kwa Yehova ? N’nali kupakila magazini kuti atumizidwe m’madela osiyana - siyana , kutumiza ena kwa anthu amene analembetsa , na kutumikila monga wolandila alendo . Kodi kukhala mpainiya kungakupatseni mwayi wocita mautumiki ena ati ? NYIMBO : 22 , 75 Ndithudi , Mulungu adzadalitsa makolo amene akuthandiza ana awo kukhala na zolinga zauzimu na kuzikwanilitsa . Yehova anauzila mtumwi Paulo kulemba kuti : “ Lamula acuma a m’nthawi ino kuti asakhale odzikweza , ndiponso kuti asamadalile cuma cosadalilika , koma adalile Mulungu , amene amatipatsa mowolowa manja zinthu zonse kuti tisangalale . Pofuna kuyamikila Yehova , Mwiisiraeli anali kupeleka nyama monga nsembe , ndipo ansembe anali kuiocha pa guwa la nsembe . N’ciani cimene mabanja angacite kuti asamalile na kutonthoza m’bululu wawo wodwala matenda osacilitsika ? 5 : 22 ) Ndipo kukhala acimwemwe kumatithandiza kupilila mavuto amene timakumana nawo mu umoyo . ( Salimo 104 : 10 - 28 ; 145 : 15 , 16 ; Machitidwe 4 : 24 ) Timayamikila cikondi cimene Mulungu amatisonyeza tikaganizila zonse zimene amaticitila kuti tikhale ndi moyo . Ndidzivutila ciani kulosela za cionongeko ngati kuti mzindawu udzaonongedwa maŵa . Ndinayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni . Pa phwando limenelo panalibe moŵa , ndipo linali ladongosolo . 1 : 17 ) Pokhala M’busa wathu , iye mwacikondi amatisamalila mwakuthupi ndi mwa kuuzimu . M’malo mwake , wacita zimenezo cifukwa waona kuti ubwenzi wathu ndi Yehova uli pangozi . Ndinabwelela ku Japan kuti ndikakonzekele . ( Luka 20 : 37 , 38 ; Aheb . 11 : 17 - 19 ) Ciyembekezo ca madalitso amtsogolo cinathandiza Mose kusaona zaka 40 za umoyo wothaŵathaŵa ndi zaka 40 m’cipululu kuti kunali kutaya nthawi . Yehova anaonetsa kuti amakonda anthu pamene analenga dziko lathu lapansi lokongola . Mukayesetsa kukulitsa makhalidwe ofunika ndi kugwila nchito mwakhama mumpingo , koma osanyalanyaza banja lanu , Yehova sadzaiŵala zonse zimene mwacita pom’tumikila . 13 : 10 ) Ena akapatsidwa udindo kapena utumiki watsopano , tiyeni tikondwele nawo . Koma Yehova anamuletsa kupitila mwa mneneli Semaya . Iye anati : “ Musapite kukamenyana ndi abale anu , ana a Isiraeli . Pofuna kuthandiza Petulo ndi atumwi enawo kuganizila zamtsogolo , Yesu anayankha kuti : “ Ndithu ndikukuuzani , pa nthawi ya kulenganso zinthu , pamene Mwana wa munthu adzakhala pampando wacifumu waulemelelo , inu amene mwatsatila ine mudzakhalanso m’mipando yacifumu 12 , kuweluza mafuko 12 a Isiraeli . “ Naphunzila kusagwedezeka pocita coyenela olo pamene kuli kovuta kutelo . NYIMBO : 77 , 59 38 : 1 , 2 , 9 - 12 . ( Sal . 37 : 1 ) Mikangano imapweteka kwambili ikacitika pakati pa abale ndi alongo . Koma munthu wodzicepetsa amatengela citsanzo ca Yesu . ( 1 Pet . 2 : 17 ) Mwacitsanzo , mlongo wina wa ku Japan anali kukhala m’dela limene linakhudzidwa kwambili ndi civomezi komanso cigumula ca madzi mu 2011 . Iye anati : “ Ndinali kudziŵa kuti maganizo anga anali onyansa pamaso pa Yehova , koma ndinali kucita mantha kwambili kuuza ena za vuto langa . ” MLONGO wina wochedwa Marilyn anati : “ Tsiku lililonse , mwamuna wanga James anali kukhala wotopa akaweluka kunchito . Nthawi zambili Samuel anali kudabwa kuti anthu akumuuza kuti amakonda kuceza mokopana ndi atsikana , ngakhale pamene sanafune kutelo . Pothela pake , anayamba kucita zimenezo mwadala . Munthu amene wadzipeleka kwa Yehova saona kuti kucita zinthu zimenezi n’kolemetsa . Mwacitsanzo : Mai wacikondi amasamalila bwino ana ake aang’ono , cifukwa mwana akakhala wamng’ono amafunikila kwambili makolo ake kumusamalila . ( Gen . 4 : 17 , 19 ) Kucokela pa Adamu kudzafika m’masiku a Nowa , ni anthu oŵelengeka cabe amene anali kulambila Yehova . ( b ) N’cifukwa ciani wophunzila afunika kukhala wokhulupilika ? Sindinakhulupilile zimene anali kukamba . Monga mmene taonela , iye sanagwilitsilepo nchito mphamvu zake kuti adzionetsele kwa ena kapena kuti adzipindulitse . ( b ) Kodi tikuphunzila ciani pa lemba la Miyambo 14 : 15 ? Ngakhale n’conco , iwo sacita zinthu mwacinyengo kuti apeze zimene afuna , koma amagwila nchito molimbikila . Mnzanu wam’cikwati , bwenzi lanu lapamtima , kapena mkulu mumpingo angakuthandizeni pa nkhawa zanu . 10 : 16 . Sitiyenela kunyalanyaza malangizo a Yehova kapena kukhumudwa ngati tikuona kuti malangizowo sanatikondweletse . M’nthawi ya Yesu , nkhani ya kupeleka msonkho inali yovuta ngako . Izi zinanithandiza kukhala womvela . 3 : 16 ) Timam’yamikila kwambili Yehova cifukwa cotionetsa cikondi copanda dyela cimeneci . A Joseph anakamba kuti : “ Poona kuti analephela kundigonjetsa , anayamba kunyengelela ana anga koma ionso anakana kucita miyamboyo . Aphunzitsiwo anali kudziŵa bwino Cilamulo ca Mose ndi miyambo ya anthu , imene inapeputsa Cilamuloco . Nanga aonetsa bwanji kuti ni wacilungamo kwambili ? Mfumu yacikanani dzina lake Yabini anayamba kuwalamulila kudzela mwa mkulu wa asilikali , Sisera . Cifukwa ca zimenezi Paulo analimbikitsa Timoteyo kuti , “ thaŵa zilakolako zaunyamata . ” ( 2 Tim . OLOŴETSEDWAMO : Yehova ndi Yesu Iye anakambanso kuti : “ Amene amapindula si aja okha amene timaphunzitsa . Kudzafika mu September , Aroma analanda mzinda na kacisi wake , ndipo anaushoka na kuupasula , osasiya mwala pa mwala unzake monga mmene Yesu analoselela . ( Mlal . 4 : 6 ) Ana amene amakonda makolo ao amayesetsa kucita zimene angathe , koma nthawi zina nchito yowasamalila ingakule kwambili . Ngati munthu alibe cikondi , amakhala wansanje , wonyada , wodzikonda , waukali ndi wosakhululukila ena , ndiponso amacita zinthu zosayenela . Tisanabatizidwe , ambili a ife tinafunika kusintha umoyo wathu kuti tizicita zimene Baibulo limakamba . Daniel , amene tamuchula poyamba paja anamvetsa mfundo imeneyi . Armen , wa ku Armenia , anati : “ Banja langa linandipempha kuti ndileke kukoka cifukwa linali kuvutika ndi fodya . Cifukwa cakuti “ Mulungu sangayesedwe ndi zinthu zoipa ndipo iye sayesa munthu ndi zinthu zoipa . ” Zimenezi zinapangitsa kuti abale ake azimucitila nsanje . ( Bokosi ) Iye sanatsatile citsanzo coipa ca atate ake . 3 : 13 - 17 ) Yesu sanacitepo chimo , conco sanafunikile kulapa . Apa , Rute anafunika kusankha mwanzelu ngakhale kuti zinali zovuta . Monga Mfumu kumwamba , saleka kutionetsa cifundo cake . Kupitila mwa mneneli Yesaya , Yehova Mulungu anati : “ Anthu awa ayandikila kwa ine ndi pakamwa pao pokha , ndipo andilemekeza ndi milomo yao yokha koma mtima wao auika kutali ndi ine . ” Anthu amenewo anataya mwayi waukulu . N’cifukwa cake Mau a Mulungu amati : “ Pamene pali nsanje ndi mtima wokonda mikangano , palinso cisokonezo ndi zoipa zamtundu uliwonse . ” — Yak . Tisalole kupanda ungwilo kwa abale athu kutilekanitsa ndi Mulungu amene timam’konda ndi kum’lambila . ( Aroma . ( Mateyu 28 : 19 , 20 ) Zonse zimene Yehova ndi Yesu amatiuza kucita zimatipindulitsa . Atangotsiliza nchito imene anapatsidwa , anali wokondwa kubwelela pamalo ake akale . — Ower . Mu 1942 , mumpingo wa Karítsa munali abale na alongo 9 acicepele a zaka za pakati pa 15 ndi 25 . Ndiye cifukwa cake , tifunikila kupeleka lipoti lathu la mu ulaliki . Iwo angacite bwino kutsatila citsanzo cabwino ca Solomo . Iye anaonetsa kulimba mtima mwa kupanga zosankha mwanzelu zokhudza nchito yomanga kacisi . Kodi adzaligwitsilanso nchito liti ? Kodi ndi mfundo ya coonadi iti imene Yesu Kristu Mfumu ya Nkhondo ikufuna kuti anthu onse adziŵe ? Iye anakulila ku Harana , mumzinda wa Mesopotamiya . Panthawiyo , tinali ndi mwana wina wamkazi , ndipo zinali zokondweletsa kuphunzila kuti banja lathu lingathe kukhala ndi moyo wamuyaya m’paladaiso padziko lapansi . Atatsiliza kukamba , zinali zopepuka kukamba naye mwacikondi . Izi zingapangitse umoyo kukhala wovuta kwa ise . Yehova akukupemphani kumuyandikila ? Ngati timacita conco , tikhoza kuphonya mfundo zina zimene zingatipindulitse . Kuganizila zabwino zimene Yehova waticitila , kudzatithandiza kupewa makhalidwe amene iye amadana nawo . Iye anali kuphunzila zimenezi ku nyumba pamene anali wacicepele komanso ku sunagoge . Nthawi zambili , pamene mumagwila bwino nchito zimene mwapatsidwa , mumapindulitsanso ena . Zoonadi , panthawi za mtendele timatha kulalikila uthenga wabwino kwa anthu ambili . ( a ) N’ciani cimakucititsani cidwi mukaganizila kukhulupilika kwa Yobu ? 3 : 14 ) Kuganizila mayankho a mafunso amenewa kudzatithandiza kupitiliza kudziyesa kuti tidziŵe kuti ndise anthu otani . Kodi pemphelo la Yona litiphunzititsa ciani ? Ndinali kuyembekezela mwacidwi kukhala kunyumba ya masisitele cifukwa ndinali kukonda Mulungu kwambili . Jennifer anaonjezela kuti : “ N’zokondweletsa kwambili kudziŵa kuti Yehova amayamikila nchito iliyonse imene timacita , ndi kuti iye sadzaiwala nchitoyo . ( Aheb . 13 : 17 ) Komanso , tidzacita zinthu mosamala kuti ‘ tisapitilile zinthu zolembedwa . ’ ( 1 Akor . ( 2 Tim . 3 : 1 - 4 ) Cikondi cadyela cimeneci n’cosagwilizana na cikondi cacikhristu . N’zoona kuti zocitika mu umoyo zingasokoneze mapulani athu . Kale , anthu ambili anali ndi mwai woona ndi kumva za mmene Mulungu anali kuthandizila Aisiraeli . 7 , 8 . ( a ) Fotokozani zimene Elisa anacita pofuna kuthetsa cisoni cimene mzimayi wina anali naco . ( b ) Kodi cozizwitsa cimene Elisa anacita citsimikizila ciani ponena za Yehova ? Yehova anakamba kuti akulu ni “ malo ousapo mvula yamkuntho . ” Jaime anayamba kupezeka pa misonkhano yacikristu , ndipo anacita cidwi ndi cikondi cimene Akristu oona ali naco . Zaka pafupi - fupi 4,000 zapitazo , wacicepele Yosefe anagulutsidwa ndi abale ake . Kuti aikebe maganizo awo pa colingaci , anamatika fomu yofunsila utumiki wa pa Beteli pa cipupa m’nyumba mwawo . ( Mat . 11 : 25 , 26 ) N’cifukwa ciani Yesu anacha ophunzila ake kuti tiana ? Ngakhale kuti panali mavuto amenewa , makadi a ulaliki anathandiza ofalitsa kulalikila anzao ndiponso anawadziŵikitsa kuti ndi alengezi a Ufumu . Ndinapitiliza kufunafuna Mboni koma sindinazipeze . Malangizo amene amapezeka m’zofalitsa zathu okhudza mmene tingacitile umboni ndi othandizadi . Ngati n’conco , munacita bwino kwambili . Zaka zotsatilapo , panapangidwa makonzedwe akuti pamisonkhano yacigawo pazikhala kafiteliya . Cifukwa codwala , banja lina ku Poland , linayamba kucita ulaliki wa makalata . 2 : 5 ) Zimenezi zinalimbitsa cikhulupililo ca Nowa . Pambuyo pake , n’nasamukila ku Melbourne , m’dziko la Australia pamodzi ndi anthu ena a m’dziko lathu . Anthu amenewa amacita cidwi na mmene zinthu za m’cilengedwe zinapangidwila , cakuti ena amapanga zinthu motengela ku cilengedwe . Ambuya anga amenewa anaphunzitsa anthu ambili coonadi , kuphatikizapo Gertrude Steele , amene anatumikila monga mmishonale kwa zaka zambili ku Puerto Rico . Kodi banja lacikristu liyenela kutsimikiza ciani posankha mmene lingasamalile makolo okalamba ? Ni mavuto aakulu ati amene Danieli ndi anzake atatu anakumana nawo ku Babulo ? Pewani kukhala cete pofuna kukhaulitsa mkazi wanu . Nanga n’ciani cimene Yobu analakwitsa ? Ni zinthu zina ziti zofunika zimene tingacite zoonetsa kuti timacilikiza ulamulilo wa Yehova ? “ Mulungu wakumwamba adzakhazikitsa ufumu umene sudzawonongedwa ku nthawi zonse . Kucita Zimene Yehova Watilamula Kumabweletsa Madalitso ( O . Tonsefe tiyenela kuivomeleza mfundo imeneyi . Pa cifukwa cimeneci , omasulila analoledwa kumasulila mau Aciheberi akuti “ Shelo ” ndi mau Acigiriki akuti “ Hade ” kuti “ Manda . ” Koma m’kupita kwa nthawi , mantha anathelatu . ( Chiv . 6 : 2 ) Yehova adzaononga dongosolo lonse la Satana padziko lapansi ndipo Satana ndi ziŵanda zake adzalandidwa mphamvu . Kodi Mboni za Yehova Zimakhulupilila Yesu ? Tiyeni tione mmene wa Mboni za Yehova angacezele ndi munthu wina . Munalinso Mboni za Yehova 7 , zimene zinamangidwa cifukwa cokana kutengako mbali m’ndale . KAKAMBIDWE : Muzikamba mokoma mtima Nanga kudziŵa zimenezi kukucititsani kumva bwanji ponena za iye ? Mwacionekele , palibe mbadwa yopanda ungwilo ya Adamu imene ikanatha kupeleka nsembe imeneyo . Dziko lapansi , ndi zonse zili mmenemo , linali kudzakhala malo awo okhalamo a muyaya . — Sal . Koma zoona n’zakuti mapulaneti amazungulila dzuŵa . Koma ngati zimene io amanena n’zosadalilika , ndiye kuti ciphunzitsoco n’cabodza . Kodi ndodo ziŵili zinaikiwa liti pamodzi ? 1 : 8 ) N’zoona kuti ambili a ise timakhala otangwanika kwambili . Wophunzila Yakobo analemba kuti : “ Mphatso iliyonse yabwino ndi yangwilo imacokela kumwamba , pakuti imatsika kucokela kwa Atate wa zounikila zonse zakuthambo . ” ( Yak . Koma mafupa a miyendo yake akathyoka , sanali kukwanitsa kupuma ndipo anali kufa mwamsanga . Liu lakuti “ ndiyeno ” n’limene linaseŵenzetsedwa mu Baibulo la Dziko Latsopano lokonzewanso mu 2013 komanso m’Mabaibo ena . Mofananamo , Yehova amakondwela tikadzipatulila kwa iye , ndipo adzatidalitsa . — Sal . McLain ) , Oct . ( Mateyu 26 : 26 - 28 ) Panganoli linatsegula mwai kwa ophunzilawo ndi anthu ena ocepa wokakhala mafumu ndi ansembe kumwamba pamodzi ndi Yesu . ( a ) N’ciani cimatisonkhezela kulalikila anansi athu ? Atapemphela , mtima wake unakhala pansi . Zimenezi zinathandiza kuti abale azitha kuphika zakudya zokwanila anthu 30,000 pa ola limodzi . NYIMBO : 23 , 138 ( Miy . 18 : 24 ) Mwacitsanzo , pamene Paula anali na zaka 5 , amayi ake anasiya coonadi . Conco , aliyense anamaliza msonkhanowo ali ndi madzi ambili akuuzimu ndiponso madzi enieni . Ndiyeno asilikali akalanda mzinda , anali kutenga ciliconse cimene afuna , kuphatikizapo cakudya ciliconse cimene catsala . Tidzapindula ngati tiphunzila nkhani za conco pa Kulambila kwa Pabanja . Mngelo anafotokoza kuti : “ Pita Danieli , pakuti mawuwa asungidwa mwacinsinsi ndipo atsekedwa ndi kumatidwa kufikila nthawi yamapeto . ” 27 : 11 ) ‘ Nanga Satana anamva bwanji ? N’cifukwa cake anati : “ Pamene ndili wofooka , m’pamene ndimakhala wamphamvu . ” ( 2 Akor . Kodi mudzakhala na moyo wautali , kapena mudzafa mwadzidzidzi ? Mwa ici , ena amaganiza kuti anthu amene anafa asanabatizike amakaponyedwa m’moto ku helo , kapena kuti amazunzidwa mwanjila ina . 4 : 31 - 34 ) Kukonda Mulungu ndi anthu kunacititsa Yesu kukhala wacimwemwe . Kuti ateteze ndi kupitiliza kulamulila nzika zake , dziko la Roma linali ndi gulu la nkhondo la mphamvu . Iye anacita izi cifukwa cakuti mlongosi wake anali atacotsedwa mumpingo cifukwa ca khalidwe la ciwelewele . Nayenso Yehova amakondwela kwambili tikadzipatulila kwa iye na mtima wonse . — Eks . Iye anafa kuti abwezeletse moyo wa anthu mmene unafunika kukhalila . Mulungu atalenga anthu aŵili oyambilila , anakamba kuti : “ Mwamuna adzasiya bambo ake ndi mayi ake , n’kudziphatika kwa mkazi wake , ndipo iwo adzakhala thupi limodzi . ” ( Gen . Anthu ambili anabatizidwa ndi mlaliki Filipo , koma io sanalandile mzimu woyela nthawi imeneyo . Baibulo limati : “ Ana a Isiraeli anakweza maso ao ndipo anaona Aiguputo akuwathamangila . Koma kuti cikwati cao cikhalitse , io ayenela kulimbitsa cikondi cao monga lawi la moto limene silizima . — Maliko 10 : 6 - 9 . Mukaunika kutsogolo , mukwanitsa kuona bwino - bwino zinthu zimene zili patali kwambili . Kodi Mau a Mulungu amatilangiza ciani pa nkhani yolamulila mkwiyo ? Cifukwa cimodzi n’cakuti asayansi na akatswili ena amalimbikitsa mfundo yakuti kulibe Mulungu , na kuti zinthu zonse zinakhalako mwa kusandulika . Koma Yehova angakupatseni nzelu kuti muthe kupilila . Ngakhale zioneke kuti uthenga wa Ufumu umene timalalikila suwafika pa mtima anthu , sitiyenela kudelela mphamvu ya uthenga umenewu . Pokamba na anthu ake , Yehova anati : “ Amene akukukhudzani , akukhudza mwana wa diso langa . ” — Zek . Nanga n’ciani cidzacitikila anthu a Mulungu panthawiyo ? 3 : 12 - 14 ) Pankhani ya apainiya aŵili amene atumikila kwa nthawi yaitali , mkulu wokoma mtima anawathandiza kuganizila mafunso aya : ‘ Kodi m’poyenela kuti ise aŵili tizikhumudwitsa ena cifukwa ca kukangana kwathu ? MFUNDO YA M’BAIBO : “ Cikondi n’coleza mtima ndiponso n’cokoma mtima . ” — 1 Akorinto 13 : 4 . Munthu winanso anaganiza zogulitsa malo ake , ndipo analimbikitsa anzake kucita cimodzi - modzi . Popeza ndife atumiki a Yehova , timalakalaka kuona cifunilo ca Mulungu ‘ cikucitika , monga kumwamba , cimodzimodzinso pansi pano . ’ Cizindikilo cimeneco cimene ciphatikizapo zinthu zimene zikuipilaipila m’dzikoli ndiponso nchito yolalikila Ufumu padziko lonse , cikuonetsa kuti tikukhala m’nthawi ya “ mapeto a nthawi ino . ” Analimbikitsanso mkazi kuti ayenela kukhala woleza mtima . Ndipo panthawi imeneyo , umoyo unali wovuta ku Kanani . sangakhale mabwenzi a Mulungu cifukwa amadziona kuti ni odetsedwa komanso ocimwa . Iye akanafunsa Yeremiya , mmodzi wa aneneli okhulupilika . Fotokozani kusiyana kumene kulipo pakati pa ulamulilo wa Yesu ndi ulamulilo wa anthu . ( 2 Mbiri 34 : 31 ) Akali wacicepele , iye “ anayamba kufunafuna Mulungu wa Davide , ” ndipo pamene anakwanitsa zaka 20 , anayamba kucotsa zinthu zokhudzana ndi kulambila mafano mu Yuda . N’cifukwa ciani anthu a Mulungu afunika kukhala ogwilizana ? Pambuyo pake , Yehova anakamba ndi amuna ena monga Mose , Samueli , ndi Davide . Pakapita masiku atatu , Farao akutulutsa n’kukudula mutu . Adzakupacika pamtengo , ndipo mbalame zidzadya nyama yako ndithu . ” Njila imodzi imene tingakhalile pamtendele ndi Mulungu ndiyo kukhulupilila nsembe ya Yesu , ndi kumvetsetsa kuti magazi ndi amtengo wapatali kwa Mlengi wathu . — Akol . Tifunika kukonda kwambili abale athu tsopano cifukwa cikondi cimeneci cidzatithandiza kupilila ziyeso zilizonse zimene tingakumane nazo mtsogolo Mzimu wa dzikoli umacititsa kuti anthu agone kuuzimu . Ndipo ngati timvetsetsa bwinobwino zimene Yehova amakonda ndi zimene amadana nazo , cidzakhala copepuka kusankha bwino mabuku , mafilimu , kapena magemu . Iye analumbila m’dzina la Yehova kuti adzakhalabe wokhulupilika kwa mfumu ya Babulo . ( Yohane 1 : 1 - 3 , 18 ) Ponena za Yesu , mtumwi Paulo anati : “ Kudzela mwa iye zinthu zina zonse zinalengedwa , zakumwamba ndi zapadziko lapansi . Inde , zinthu zooneka ndi zinthu zosaoneka , kaya ndi mipando yacifumu , kapena ambuye , kapena maboma , kapena maulamulilo . Conco , lekani kuti kutumikila Yehova kukhale kokondweletsa kwa inu , mosasamala kanthu za udindo umene muli nao . Iye anakamba kuti mwamuna wake anaona kuti nchito yake inali kuika ubwenzi wao ndi Yehova pa ngozi . Enoki anali ndi cikhulupililo ngakhale kuti anali kukhala ndi anthu osaopa Mulungu amene anali kukamba zinthu zonyoza Mulungu . M’bale Jensen anali kudziŵa bwino nchito yoniyenelela . M’bale wina dzina lake Jesús , amene anali kukhala ku Mexico anati : “ Ndinakhala kapolo wa nchito yanga , ndipo nthawi zina ndinali kuseŵenza maola ambilimbili ngakhale sanandiuze kutelo . 1 : 2 , 3 . Ndipo tiyeni tionetse Yehova kuti ndife oyamikila potitsogolela ndi kudalitsa nchito yathu yophunzitsa padziko lapansi . Ndi mwai wotani umene atumiki a Yehova akhala nao nthawi zonse ? Kodi cikondi ceni - ceni cimalimbikitsa munthu kucita ciani ngati wacita chimo lalikulu ? Nthawi imeneyo inafika pamene Yesu anapeleka nsembe imene inathetsa njila imene Ayuda anali kulambilila yozikidwa pa Cilamulo ca Mose . Kodi atsogoleli a anthu a Mulungu akale komanso Yesu Khiristu anaonetsa bwanji kuti anali . . . Nkhani yaciŵili ifotokoza zimene anthu otumikila mumpingo wa cinenelo cina angacite kuti akhalebe auzimu . Colinga cacikulu cimene timapezekela pa misonkhanoyi ni kulambila Yehova . Umoyo uli monga ulendo , ndipo acicepele ali ngati anthu amene ali pa sitesheni ya basi . Yohane anakamba mau akuti “ okana Kristu ambili , ” kuonetsa kuti wokana Kristu si munthu mmodzi koma ndi gulu la anthu . M’malomwake , timaugwilitsila nchito mosamala . Panthawiyo ndinalibe ndalama zokwanila . Kodi inu muona kuti mungakwanitse kucita zambili potumikila Yehova ? M’malomwake , tiyeni ‘ tikhulupilile Yehova ndi mtima [ wathu ] wonse . ’ — Miy . ( Onani bokosi lakuti “ Maphunzilo Anu a Baibulo Ofunika Kwambili . ” ) kukonda cuma ? Yosefe anafotokoza zimene Farao angacite . “ Yehova anathetsa masautso a Yobu . . . . Komabe , patapita maola angapo , ndinayamba kunjenjemela ndi mantha . ” — Alona , wa ku Israel . Mpaka pano mfundo imeneyi yakhala yothandiza . — Levitiko , caputa 13 na 14 . Mafunso amenewa adzayankhidwa m’nkhani yotsatila . Ngati makolo okalamba ndi ana akhala motalikilana , zingakhale zovuta kwa ana kupeleka cisamalilo coyenelela . Munthu wina pokondwelela kuti watha caka osatambako zamalisece , analemba kuti : “ Poyamba n’nali kudziona ngati wacabe - cabe , koma tsopano nimadziona kuti ndine munthu . ” Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa ndi yakale kwambili , ndipo inalembedwa zaka 1,000 malemba a Ciheberi olembedwa ndi Amasorete asanalembedwe Atumiki a Yehova amayesetsa kukonza zinthu zoonongeka pa malo olambilila . Conco , gulu la Mulungu limayesetsa kupeza njila zocepetselako ndalama zowonongedwa , komanso limapepukitsako nchito zina , n’colinga cakuti likwanitse kucita zambili poseŵenzetsa zopeleka zanu zimene mumapeleka mowolowa manja . Ku Beteli , n’nali kugwila nchito zosiyana - siyana , monga ya mu ofesi , yolonga mabuku , yophika , ndi yoyeletsa . 1 Akor . 13 : 7 , 8 ) Akhiristu oopa Mulungu sayenela kuiŵala lumbilo lawo lakuti adzakondana ndi kukhulupilika kwa wina ndi mnzake . Ici cidzawathandiza kugwilitsila nchito malangizo apamwamba a Yehova pofuna kuthetsa mavuto alionse amene angabwele . 12 , 13 . ( a ) Kodi atumwi anacita ciani pamene Yesu analalikila mayi wacisamariya ? 19 : 28 - 30 . Kodi anyamata mukumva bwanji kudziŵika ndi dzina la Yehova ? Kodi Baibulo limati “ mapeto ” n’ciani ? 4 : 7 - 9 . ( Mateyu 22 : 39 ) Ngati ticita zinthu zimene zingaike ena pangozi ndiye kuti sitikonda anansi athu . 1 , 2 . ( a ) Kodi Yehova watipatsa zinthu zitatu ziti zimene ndi cuma cauzimu ? Mlongo Heidi , wa ku Germany , wa zaka za m’ma 70 , watumikila ku Ivory Coast ( lomba lochedwa Côte d’Ivoire ) kucokela mu 1968 . Mavuto a kudwala ( Onani palagilafu 15 ) Khiristu na angelo ake ali pafupi kuwononga dziko loipali . Mwa ici , galeta ya Yehova ili pa liŵilo ! Nkhani yaciŵili idzafokoza zinthu zimene okwatilana ayenela kucita kuti cikwati cao cikhale colimba mwakuuzimu . Iyai , simuyenela kuganiza conco . Iwo atumikila mumpingo wa anthu osamva , ndipo amacilikiza mpingo wa cinenelo ca manja pothandiza ofalitsa osamva ndi ena a cidwi 300 a m’dzikolo . Yelekezelani kuti muli pa ulendo . ( Yeremiya 29 : 12 ) Ngati mumakamba ndi Mulungu , ‘ mumamuyandikila ndipo iyenso amayandikila kwa inu . ’ Kodi sicokondweletsa kuona mmene Yesu anagwilitsila nchito mphamvu zake zozizwitsa posamalila amuna ndi akazi , kuphatikizapo ana ang’ono ? ( b ) Ndi funso liti limene lidzayankhidwa m’nkhani yotsatila ? Mabaibo amenewo anali ang’ono - ang’ono . Cifukwa cakuti anali ang’ono - ang’ono , anali ochipa kusiyana ndi Baibo ikulu . Koposa zonse , popemphela n’nali kuuzanso Yehova za colinga canga . ” ( Aef . 6 : 2 - 4 ) Mwacitsanzo , kodi mungafune kukhala ndi mmodzi wa ana anu ndi banja lake ? Ndinali kufuna kutumikila Yehova ndi moyo wanga wonse , koma ndinali kukondanso kwambili acibale anga . Poyamba ndinali kuwasoŵa kwambili acibale anga . Mukacita zimenezo , mudzalimbikitsidwa kucita zinthu zoonetsa kuti mumayamikila mphatso yapadela imeneyo . Fotokozani citsanzo coonetsa kuti m’pake ufulu wathu kukhala na malile . Koma m’kupita kwa nthawi timangozindikila kuti mbeu za Ufumu zimene tinabyala zabala zipatso . Nanga anali kutanthauza ciani ? Yehova sanam’dzudzule Elihu pamene anafunsa kuti : “ Ngati ndinudi wosalakwa , kodi mumam’patsa ciani [ Mulungu ] ? Kodi Yehova waonetsa bwanji kuti “ ndi amene anayamba kutikonda ” ? 27 Mbili Yanga ​ — Masisitele Anakhala Paubale Weniweni Wakuuzimu Zitsanzo za conco zimaonetsa kuti mfundo za m’Baibulo n’zothandizadi . — Aheb . Zinthu zamtengo wapatali ndiponso cuma zili m’nyumba yake , ndipo cilungamo cake cidzakhalapo kwamuyaya . ” ( Sal . M’bukuli , muli mfundo zothandiza kwa munthu aliyense . ” Mwacitsanzo , amai anali kundiletsa kuphunzila , ndipo nthawi zina anali kundinyengelela kuti ndisiye . ( Miyambo 4 : 5 - 7 ) Mwacitsanzo , iye amafuna kuti tiziuzako ena ‘ coonadi colondola ’ ndi kuwathandiza kuti akapulumuke . Iyai . Mulungu amakhululukila anthu okhawo amene amalapa kucokela pansi pa mtima . Mavesiwa akupezeka pa 1 Samueli 2 : 25 ; 6 : 3 ; 10 : 26 ; 23 : 14 , 16 . Kodi kuphunzila Baibo kungatithandize bwanji kukhala odziletsa ? N’cifukwa ciani anabwelela ? Iye sanafune kuti anthu azifa . NJILA YOTHETSELA VUTOLI : Mulungu anasankha Yesu Kristu kukhala Wolamulila wa Ufumu wake . Komanso anali kukonda kwambili amishonale padziko lonse lapansi . Ayenela kumvetsetsa zimene amaŵelenga ndi kuzigwilitsila nchito . Nanga kucita zimenezi kuphatikizapo ciani ? Lonjezo lofunika kwambli limene Mkhristu angapange ni la kudzipeleka kwa Yehova . Ndipo mwininyumba sangaike ziwiya za conco pamodzi ndi ziwiya zaukhondo , monga ziwiya zophikila . Pa cifukwa cimeneci , Yehova anapeleka ciweluzo kwa Zedekiya mwa kunena kuti : “ Pali ine Mulungu wamoyo , [ Zedekiya ] amene ananyoza lumbilo ndi kuphwanya pangano limene anacita ndi mfumu imene inamulonga ufumu , adzafela m’dziko la mfumu yomweyo , dziko la Babulo . ” — Ezek . Pamene ticita zimene tingakwanitse kuti titumikile Mulungu , ‘ timalaŵa ndi kuona kuti Yehova ni wabwino . ’ Kodi ‘ ndidzathandiza ndi kulimbikitsa ’ mpingo ? — Akol . Umoyo wa Aisiraeli unali kutsogoleledwa ndi Cilamulo ca Mose kwa zaka zopitilila 1,500 . 22 : 15 ) Iwo angakambe kuti , ‘ Popeza mwana wanga akali wosabatizika , sangacotsedwe . ’ Savutikanso kulandila maganizo a ena ndi atsopano . Anthu amene ndi mbeta ndi ofunika mumpingo , ndipo nthawi zambili amathandiza mabanja ndi acicepele Ukatelo udzayenda panjila yako popanda cokuopseza , ndipo ngakhale phazi lako silizapunthwa ndi ciliconse . ” Ndi nzelu zotani zimene Yehova watipatsa zimene zingatithandize kuti timutsanzile ? Wophunzila Yakobo anakamba kuti : “ Ndikuonetsa cikhulupililo canga mwa nchito [ zanga ] . ” Pelekani zitsanzo . ( b ) Kodi mukuphunzila ciani pa zimene abale ena anacita pamene kunacitika ngozi zacilengedwe ? Mwezi umodzi m’mbuyomo , akawalala asanamubele , Riana anali atayamba kuphunzila Baibo na amuna aŵili a mtundu wa Antandiroyi . Anakambanso kuti : “ Tinaphunzitsa ana athu kumene angapeze thandizo labwino kwambili akakhala ndi mavuto . Ananiuza kuti : “ Andreas , ngati ufuna kupeza mayankho pa mafunso ako okhudza moyo na tsogolo , uziŵelenga Baibo mwakhama . ” Tinayamba kulembelana makalata . N’nali kumufotokozela zokhudza mpingo wathu . Nayenso anali kunifotokozela za mmene nchito yolalikila inali kupitila patsogolo ku Boston . ( Aheb . 13 : 15 , 16 ) Nsembe zimenezi zimabweletsa cimwemwe na madalitso , monga mmene tidzaonela m’zitsanzo zotsatila . Ngakhale n’conco , iye anaonetsa kuti anali na “ mtendele wa Mulungu . ” Popeza cikhulupililo ni khalidwe limene mzimu woyela umatulutsa , tifunika kupitiliza ‘ kupemphabe ’ mzimu wa Mulungu monga mmene Yesu anatiuzila . — Luka 11 : 9 , 13 . Kodi palinso zina zimene tingaphunzile kwa Mose ? Inde . Caciŵili , zimene Yehova akutiphunzitsa pali pano , akutikonzekeletsa kukakhala bwino m’dziko latsopano . ( Yes . 54 : 13 ; Yoh . ( Mateyu . 4 : 8 , 9 ) Conco , pamene Satana anatenga Yesu kupita naye ku kacisi , n’kutheka kuti anafunadi kuti Yesu aike moyo wake pa ngozi mwa kumuuza kuti adziponye pansi kucokela pamwamba pa kacisi . Mofanana na wofufuza golide , kodi mumayesetsa kuphunzila mfundo zamtengo wapatali za coonadi ca m’Baibulo ? Matthew wa zaka 34 ndi m’bale wake Michael wa zaka 28 akhala ku Canada . Pambuyo pa caka cimodzi , n’nafunsila upainiya wanthawi zonse . Anthu ambili anamwalila asanadziŵe coonadi ca m’Baibulo . Yesu . ( Ŵelengani Mateyu 25 : ​ 8 , 9 . ) Angacite zimenezi cifukwa coganiza kuti sipanacitike cilungamo , kapena cifukwa congofuna kuti papiteko kanthawi munthuyo asananyongedwe . N’cifukwa ciani kuganizila za ciyembekezo cathu mwapemphelo n’kopindulitsa ? 10 : 24 ; 13 : 5 ) Kuwonjezela apo , munthu wacikondi , amaganizila ena , amakhala woleza mtima , komanso wokoma mtima . Komabe mwina ife tingadzafunike kuyembekezela kwa kanthawi kuti okondedwa athu aukitsidwe . Ngakhale kuti ndife opanda ungwilo , n’zotheka kumvela Mulungu . Timayesetsa kukhala mwamtendele ndi abale na alongo athu ngakhale pamene atilakwila . Aisiraeli anafunikilanso kuphunzitsa ana ao kutsatila miyezo yoyela ya Mulungu . Tizikumbukila kuti cimene cidzatikweza si maluso athu , koma kudzicepetsa kwa Yehova . ( Sal . ( Yeremiya 10 : 12 ) Katswili wina wa Baibulo anati : “ Dziko lapansi linalengedwa mwaluso kwambili n’colinga cakuti anthu azikhalamo . ” [ Cithunzi papeji 3 ] [ Eni ake ] Strdel / AFP / Getty Images [ Cithunzi papeji 4 ] [ Eni ake ] N’zacisoni kuti anthu ena amaona kuti Mulungu sangawakonde . Koma maumboni ena anaonetsa kuti nthawi zina zingatheke dzila la mkazi kulumikizana ndi mbeu ya mwamuna . Koma tiyeni tionetse kuti cinthu cofunika kwambili pa umoyo wathu ndi kukhala okhulupilika kwa Yehova . Paulendo wina tili ku Brooklyn zaka zambili zapitazo , ine na mkazi wanga , Mary , tinaceza ndi M’bale Franz na abale ena m’madzulo . Anthu amene amakudziŵani bwino angakulangizeni mwanzelu . Mavuto ambili amene acinyamata amakumana nao olembedwa m’nkhani zimenezi amakhudza Akristu onse . 4 : 10 ) Kumbukilani kuti kwa kanthawi Sauli anali kucita bwino ndipo Mulungu anamukonda , koma analephela kuthetsa mzimu wodzikonda umene anayamba kukhala nao . Ndiponso , si canzelu kutumila ena nkhani zimene mwajambula , kapena mfundo zonse zimene mwalemba zokhudza nkhani za Baibulo . Anthu amakopeka nafe cifukwa ca “ mzimu wabata ndi wofatsa , ” osati kudzitama kapena kudzionetsela iyayi . ( Chivumbulutso 14 : 1 ) Pamene Yesu anali padziko lapansi , nkhani yaikulu imene anali kuphunzitsa inali yonena za Ufumu . Iye anaphunzitsa ophunzila ake kupemphela kuti : “ Atate wathu wakumwamba , dzina lanu liyeletsedwe . Tiyenela kudzifunsa mafunso ati pankhani ‘ yomvela mocokela pansi pa mtima ’ ? NYIMBO : 136 , 129 Ngati nyumbayo ndi imene mukukhalamo , mukhoza kuipeleka koma n’kupitiliza kukhalamo pa nthawi yonse imene muli na moyo . 3 : 1 ) Pa zinthu zimene tachulazi , kodi pali cimene muona kuti mufunika kuongolela ? Iye anali kudziŵa kuti posacedwa , nayenso adzapita kumeneko . ( Mlal . 18 : 2 ) Pa cifukwa ici , zocita zathu zimasiyana ndi za anthu a m’dzikoli , ndipo izi zacititsa kuti ena azitinyoza . Ku Mexico , anthu ambili amakamba Cisipanishi , koma kulinso anthu ocepa amene amakamba zinenelo zina . Ngakhale n’conco , sitiyenela kuiŵala colinga cimene Yehova watipatsila ufulu umenewu . PAMENE n’nali ndi zaka 12 , n’nazindikila kuti nili na cinthu camtengo wapatali cimene ningapatseko ena . ( a ) Kodi Yehova anagwilitsila nchito cinenelo citi pokamba ndi Mose , Samueli , ndi Davide ? Buku yakuti A Lawyer Examines the Bible inati : “ Nkhani zacikondi , nthano , ndi maumboni abodza , zimalembedwa mosamala kwambili kuti zigwilizane ndi zocitika komanso nthawi ya kudela linalake , . . . koma nkhani za m’Baibo zimachula ndendende deti ndi malo kumene zinthuzo zinacitikila . ” Koma kodi tonse tingapindule bwanji mwa kuŵelenga nkhani ndi mabuku amenewa ? Yehova akanafuna akanayambila kuchula za mphamvu kapena nzelu zake . N’cifukwa ciani anacita zimenezo ? Yesu anali kudziŵa bwino mau a Mulungu . Ndiye cifukwa cake iye atakumana ndi ciyeso anayankha mwamsanga pogwilitsa nchito malemba . Ndiponso , Mulungu ali ndi mphamvu ndipo angasinthe zinthu kuti zimene walosela zikwanilitsike mmene iye afunila . Iye anadabwa atadziŵa cifukwa cake : Atate wake analimbana ndi mngelo wamphamvu usiku wonse ! BAIBULO limafotokoza kuti madela ena a Dziko Lolonjezedwa anali ndi nkhalango zoŵilila . ( 1 Maf . ( 1 Akor . 6 : 9 , 10 ) Tisawonjezele mayeselo kwa iwo . Iwo akukonzekeletsedwa za moyo wa m’paladaiso padziko lapansi . — Mlaliki 12 : 13 ; Mateyu 22 : 37 - 39 ; Akolose 3 : 15 . A Daka : Iyai . Ngati m’bale aoneka kuti safuna kukalamila maudindo , n’zotheka kumuthandiza kusintha maganizo koma pamafunika khama ndi kuleza mtima . Matthew anati : “ Nkhaniyo itatha , sindinaleke kuganiza za ku Russia . Conco ndinapeleka pemphelo lacindunji kwa Yehova kuti andithandize kukwanilitsa colinga canga cokatumikila kumeneko . ” NYIMBO : 76 , 141 Timazindikila ise , abale athu ndi alongo athu , tonse ndise opanda ungwilo . Colinga cathu cacikulu poseŵenzetsa mphatso ya ufulu wocita zinthu , ndico kuonetsa cikondi cathu kwa Mulungu , ndi kuti ulemu ndi ulemelelo wonse zipite kwa iye . Iye anali kuda nkhawa kuti asamalila bwanji banja lake . Kodi sitiyamikila kuti Mulungu watidalitsa mwa kutipatsa mtendele waukulu wa mumtima ? ( Mateyu 6 : 33 ) Pamene ine ndi Laurie tinafika ku United States , tinaganiza zoleka kuzungulila dziko ndi kukhazikika kumeneko n’colinga cakuti tiike patsogolo zinthu zokhudza kulambila . Pamene Adamu anacimwa anataya moyo osati wa zaka 70 kapena 80 , koma wokhala kwamuyaya . M’nkhani ino , tikambilana zinthu zinai zimene zidzatithandiza kukhalabe okhulupilika kwa Yehova . M’malomwake , tiyenela kuseŵenzetsa zida zimene gulu la Yehova latipatsa kuti tiwathandize kukonda kwambili kuŵelenga Baibulo . Zilembo za Cijapanizi zingalembedwe kucoka pamwamba kupita pansi kapena kucoka kumanzele kupita kulamanja . Mabuku ambili kuphatikizapo zofalitsa zathu zaposacedwapa zakhala zikulembedwa kucoka kumanzele kupita kulamanja . Timakwanitsa kuonetsa cikondi codzimana cifukwa Mulungu anatilenga m’cifanizilo cake . Anthu anadabwa kwambili kuona Yesu ataukitsidwa pambuyo pokhala m’manda masiku atatu . ( Onani cithunzi cili kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) N’cifukwa ciani Mose sanaope mfumu ? Iwo amamvela monga mmene wamasalimo anamvelela , amene analemba kuti : “ Ndimakonda kwambili cilamulo canu ! Panthawiyo , iye anali ndi khalidwe logonana ndi akazi anzake . Akhristu ena ni osauka , ndipo amaona kuti sangakwanitse kupatsa alendo zakudya zabwino monga zimene ena amapatsa alendo . Mulungu watithandiza kukhala otsimikiza kuti zimene anatilonjeza adzazikwanilitsa . Mwacitsanzo , zinthu monga nthenda ya kukha m’thupi , khate , kapena kugwila mtembo wa nyama kapena wa munthu . Mulungu anauzila maulosi ena okhudza Timoteyo , mwina anali okamba za utumiki umene anali kudzacita pothandiza mipingo yambili . Tingatsimikize bwanji kuti Yehova adzatidalitsa ? Pa cifukwa cimeneci , timadzifunsa kuti : ‘ Kodi “ paradaiso ” ni nkhani yongolota cabe ? Nkhaniyi ifotokoza cifukwa cake zingakhale zovuta kusintha ndiponso mmene Baibulo lingatithandizile . Ngati zotelozo zikanacitika , Ayuda amene anali kugwilizana na Akhiristu akanapatsidwa cilango , ndipo akanaletsedwa kulalikila m’kacisi ndi m’masunagoge . Mu March 1965 , tinapatsidwa mwayi wotumikila mipingo m’nchito yoyendela dela . Kodi anthu ndiyenela kukambitsilana nao motani ? Marilyn anapempha ena kuti amuuzeko zocita pankhaniyi . Mwina anakumbukila mau amene ali pa Ekisodo 23 : 19 , pamene pamakamba kuti anthu a Yehova ayenela kupeleka kwa Iye zinthu zao zabwino koposa . Kodi ana anu acinyamata angapindule bwanji ngati muwafotolozela cifukwa cimene mwapangila lamulo kapena cosankha cina cake ? Ine , mkazi wanga na ana athu 8 mu 1989 141 : 5 ) Tiyelekezele motele : Tinene kuti munthu wina akudya nsima ndipo nyama yamukhala pakhosi . Onani zimene mungacite kuti muwonjezele utumiki wanu . — w16.07 , peji 10 . M’nkhani ino na zitatu zotsatila , maina ena asinthidwa . Podzafika mu June 2014 , tinali titapambana kale milandu yoposa 57 mu khoti limeneli , ndipo maiko ambili a ku Ulaya amafunikila kutsatila zigamulo zimene khotili limapeleka . ( 2 Mbiri 19 : 4 ) Mfumu Yehosafati “ anafunafuna Yehova ndi mtima wake wonse . ” — 2 Mbiri 22 : 9 . 41 : 10 ) Caciŵili , Mulungu amakukumbutsani kuti malonjezo ake ndi odalilika . Conco , zimene Yeremiya analemba zaka 1,000 Rakele atafa kale zingamveke ngati si zolondola . Pokamba na Akhristu a ku Efeso a m’zaka 100 zoyambilila , Yesu Khristu anati : “ Ndakupeza ndi mlandu wakuti wasiya cikondi cimene unali naco poyamba . ” ( Chiv . 16 , 17 . ( a ) Kodi akulu angathandize bwanji Akristu amene akuvutika kuthetsa zilakolako zoipa ? ( Muonenso kabokosi ka mutu wakuti “ Aweluzidwa Kukhala Oyenela Akafa . ” ) ( c ) Kodi amene anali kucilikiza odzozedwa adzalandila mphoto yotani ? Abale ambili amene akuthandiza pa nchito yomanga ku New York akanafuna sakanadzipeleka kuthandiza panchitoyo . Akhristu acicepele afunika kulandila malangizo kucokela kwa makolo awo . Komabe , iwo ali na udindo wopanga zosankha pa nkhani zina zofunika kwambili . Yosefe atawaona m’mawa , anadziŵa kuti cinacake sicinali bwino . ( Onani palagilafu 10 ) Aristotle anali kuphunzitsa kuti zinthu zonse za kuthambo zili mkati mwa zinthu zooneka monga mabola agilasi , ndipo dziko lapansi ndilo lili pakati peni - peni . Kudzafika ca m’ma 1700 . Koma cikhulupililo cawo mu mphamvu za Mulungu , cinawacititsa ‘ kutseka mikango pakamwa ’ ndi ‘ kugonjetsa mphamvu ya moto , titelo kukamba kwake . ’ — Aheb . Anthu ena amati ngati kutentha kupitilizabe padziko lapansi , ndiye kuti panthawi ina madzi onse oundana amenewa adzasungunukilatu cakuti sadzaundananso . Iye akusangalala ndipo akulimbikitsidwa poona kulimba mtima ndi cikhulupililo ca asilikaliwo . M’nthawi ya atumwi , Akristu anafunika kusiya katundu wao ndi kupilila mavuto ambili kuti apulumuke . Mulimonse mmene anthu amaonela uthenga wathu , ife timatsatila malangizo opezeka m’Baibulo . 19 : 6 - 8 ) Motelo , Yesu anaonetsa kuti lamulo la cikwati limene Mulungu anakhazikitsa m’munda wa Edeni liyenela kutsatilidwa mu mpingo wacikhiristu . Kodi kuganizila zimene wamasalimo anakamba pa Salimo 147 : 4 kungatipindulitse bwanji ? ( Mlal . 7 : 16 ) Akulu odzicepetsa samaona kuti amaposa Akristu ena . Ndipo caka cino ca 2014 , Ufumu wa Mulungu wakwanitsa zaka 100 kucokela pamene unakhazikitsidwa kumwamba . Tikamva kuti anthu amene tinawathandiza kuphunzila coonadi akutumikila Mulungu mokhulupilika , timalimbikitsidwa ngako , monga mmene mtumwi Yohane analimbikitsidwila . Iye analemba kuti : “ Palibe cimene cimandisangalatsa kwambili kuposa kumva kuti ana anga akuyendabe m’coonadi . ” ( 3 Yoh . N’cifukwa ciani ? Atate anga anamwalila ndi matenda a kansa . Mwacitsanzo , anthu ena m’gawo lathu angakhale kuti anacotsedwa nchito mosayembekezela ndipo ni othedwa nzelu . Zinthu ngati zimenezi zikawacitikila , anthu angayambe kudzifunsa mafunso okhudza colinga ca moyo , amene poyamba sanali kuwaganizila . imene ili mu Galamukani ! Conco , ampatuko mu mpingowo sakanalepheletsa colinga ca Yehova monga zinalili m’nthawi ya Kora . Kodi nimakondwela kwambili nikamacita zinthu ziti , zauzimu kapena zakuthupi ? ’ Uzifunsa mafunso moona mtima , ndi kukamba modzicepetsa ndi mwaulemu , maka - maka pokambilana ndi acikulile . Anatiuza kuti tikatumikile ku Cambodia monga amishonale . Rakele anamwalila ana ake aŵili asanamwalile . Pelakani citsanzo ca m’Baibulo coonetsa zimene tiyenela kucita pakakhala kamvedwe katsopano ka mfundo za m’Malemba . Kodi kumvela kugwilizana bwanji ndi kukhala oyela ? Zoonadi , cisomo ca Mulungu cimatsogolela ku ‘ moyo wosatha kupitila mwa Yesu Khiristu . ’ — Aroma 5 : 19 , 21 . May Brown , amene anali woyang’anila dela , na Fred Rusk amene anali kutumikila pa Beteli . Gwen : Kukamba zoona , zinali zovuta kuti ndizoloŵele kukhala pa famu . Ngakhale kuti kukhulupilila zakuthambo kunayamba kale - kale ku Babulo wakale , mpaka pano kukali kofala . ( Miy . 15 : 15 ) Ena amakhumudwa cifukwa ca matenda amene amawavutitsa maganizo . Tikakumana ndi zinthu zaconco , sitifunika kudzidalila , koma tifunika kudalila Yehova . Muzikhala oyela , cifukwa ine ndine woyela . ” ( Lev . 3 Njila Yopezela Ufulu Weni - weni 10 , 11 . ( a ) M’fanizo lake la tiligu ndi namsongole , Yesu anakambilatu za ciani ? Anthuwo akapita kukafunafuna ndalama sizimatanthauza kuti basi adzazipeza . Pambuyo pake , M’bale Bud Miller ndi mkazi wake , Joan , anayamba kutumikila m’dela lathu monga woyang’anila dela . Nafenso timathandiza ena ‘ kufuna - funa Yehova . ’ Pofuna kuonetsa kuti lonjezo limeneli ndi la m’Malemba , Paulo anagwila mau ena a pa Genesis 2 : 2 ndi Salimo 95 : 11 . Kuyambila nthawi imeneyo , Chechi na Boma zinayamba kuseŵenzela pamodzi . Panthawi imeneyo , iye sanathe kulamulila monga mfumu . CILENGEDWE CIKUONONGEKA PANG’ONOPANG’ONO Anthu apeleka njila zosiyanasiyana za mmene “ mavuto a mwadzidzidzi amene pulaneti ” lathu likukumana nao angathetsedwele . Posamalila okalamba amenewa ena amasinthana - sinthana . ( a ) N’ciani cakhala cikucitika kuyambila mu 1914 ? Mwacionekele , munaŵelenga ndi kusangalala kwambili na nkhani za anthu aconco zopezeka mu Nsanja ya Mlonda , za mutu wakuti “ Baibo Imasintha Anthu . ” Zimene anakamba zinangoonetsa maganizo aumunthu . Ngakhale kuti sitili pansi pa Cilamulo ca Mose , malangizo ambili opezeka m’Cilamuloci angatithandize pa umoyo wathu wa tsiku ndi tsiku ndi polambila Yehova . Mukanakhalako panthawiyo , kodi sembe munamvela bwanji ndi zocita za atumwiwo ? Kale tinali kukamba kuti munthu amene ananyamula kacikwama ka mlembi konyamulilamo inki amaimila odzozedwa amene akali padziko . Kodi inunso mumaona conco ? Mzimu wokonda dziko lako ukukulila - kulila , ndipo ambili amakhulupilila kuti kukhala na ufulu wodzilamulila kungawathandize kukhala na umoyo wabwino . Ndiponso zakuthandizani kuti mukhale “ woyenelela bwino ” kugwila nchito ya Mulungu . N’nabadwila m’mudzi winawake m’tauni ya Saxony , m’dziko limene panthawiyo linali German Democratic Republic ( GDR ) . Tingaonetse mwa zocita zathu . Koma aliyense aziganiza m’njila yakuti akhale munthu woganiza bwino . ” — Aroma 12 : 3 . Ndiyeno , ofesi ya nthambi inali kudziŵitsa bungwe la akulu za abale amene anasankhidwa . Buku lina linakamba kuti , cikondi ca a·gaʹpe “ cimaonekela kwambili mwa zimene munthu amacita . ” Mwina sitikanamvetsela , ndipo pakanafunika kuti olalikilawo aticitile cifundo . 10 : 16 ; Chiv . Koma nthawi zonse iye anali wacikondi , wokoma mtima , wololela , wofatsa , ndi wodzicepetsa . — Mat . ( Aroma 15 : 4 ) Tikamaphunzitsa anthu coonadi ca m’Baibulo , io amakhala anzathu . Munthu amakhala na cikhulupililo “ cifukwa ca zimene wamva . ” Anthu ena amamvetsela uthenga wathu koma ena samvetsela . ( 1 Yohane 4 : 8 ) Iye analenga anthu cifukwa anafuna kuti awapatse moyo monga mphatso . Iye anafotokoza mfundo imene anaphunzilapo pa lembali . Anati : “ Ni cinthu canzelu kucita zinthu mozindikila na kulinganiza bwino zinthu . Kodi zimene Baibo imakamba n’zoona ? Conco , ndi kwanzelu kukonzekela masautso pasadakhale . Amacita zimenezi cifukwa coyamikila Yehova monga Mpatsi Wamkulu . Makolo ndi acicepele amene acita zimenezi timawayamikila kwambili . — Ower . Iwo anauza aphunzitsi anga kuti akambe nane , koma sizinaphule kanthu . N’naona kuti nthawi zambili anthu amene amakonda kucita ciwawa amaphedwa . Ngati wina waleka kusambila akali kutali ndi mtunda , amamila . Baibulo yapulumuka zambili . Nkhani ya Jowana imatiphunzitsa zinthu zambili zofunika . 26 : 20 ) Panthawi yovuta imeneyo , Yehova adzatipatsa malangizo kuti tikatetezeke . Ndipo mwina ‘ zipinda zathu zamkati ’ ndi mipingo yathu . Mose akangokweza manja ake m’mwamba , Aisraeli anali kupambana nkhondoyo . 24 : 14 ; 25 : 40 . Zopeleka zimene atumiki a Mulungu anali kupeleka anali kuzipeza m’njila zosiyana - siyana . Citsanzo ca Rehobowamu , mfumu ya Yuda , cingatithandize kupeza yankho . Tiyenela kutengela zimene mtumwi Paulo ndi anzake anacita . “ Zocita za anthu zaononga pafupifupi 50 pelesenti ya nthaka yonse ya padziko lapansi ndipo zimenezi zabweletsa mavuto ambili okhudza ” nchito yoteteza ndi kusamalila zacilengedwe , zomela zimasoŵa cakudya cokwanila . . . ndiponso mavuto ena okhudza nyengo . ” — Global Change and the Earth System . Fotokozani citsanzo coonetsa kuti mau a pa Mateyu 11 : 28 - 30 ni oona . NKHANI YA PACIKUTO | KODI IMFA NDI MAPETO A ZONSE ? Muyenela kutumiza zinthuzo limodzi ndi kalata yonena kuti ndi copeleka . ( Onani mau akumapeto . ) Tiyenela kusamala kuti tisayambe kudandaula monga anchito a m’fanizo la Yesu . Ndiye cifukwa cake Yehova anamukantha ndi khate . Kuti mudziŵe zambili zokhudza nsembe ya Yesu ndi mmene ingakupindulitsileni , tambani kavidiyo kacidule kakuti Kukumbukila Imfa ya Yesu ? Mipingo yambili inali yaing’ono ndiponso yatsopano . Ndipo koposa zonse , Yehova Mulungu amakondwela nafe ndi kutinyadila . 23 : 23 ) M’malo mwake , iye mokoma mtima anamuuza kuti : “ Mwanawe , cikhulupililo cako cakucilitsa . Zimenezi zapangitsa kuti cikondi cicepe kwambili pakati pa anthu osalambila Yehova Mulungu . ( b ) Kodi kudzicepetsa kwa Yesu kunathandiza bwanji ophunzila ake ? Olson ) , 10 / 15 Ophunzila a Yesu anam’tsatila ndi mtima wonse , ndipo anatsimikiza kuti anasankhidwa ndi Yehova . Mose anauza Aisiraeli kuti : “ Yehova Mulungu wanu adzakupatsani mneneli ngati ine , kucokela pakati panu , kucokela pakati pa abale anu , ndipo inu mudzamvele mneneli ameneyo . ” Nditatsiliza kuŵelenga , ndinabwelelanso kwa wansembeyo ndi mafunso ambili . Linafotokozanso kuti kunzunzidwa kwa Naboti kumene Yezebeli anacititsa kunali kuimila kunzunzidwa kwa odzozedwa m’masiku otsiliza . Kodi anthu ambili amaiona bwanji nchito yawo ? Ndaphunzilanso kukhala wokhutila ndi zimene ndili nazo , ngakhale kuti n’zocepa . ” Dokotala wina wa ku India dzina lake Jayavanth anakoka fodya kwa zaka 38 . Koma coyamba tiyeni tikambilane mfundo za m’Baibo zimene zingatithandize kukhala na thanzi labwino . Mofanana ndi zimenezi , timafunika kudya cakudya coculuka cakuuzimu kuti tikwanitse kupilila ndi kupambana ciyeso . 21 : 8 ) Tikaona mapindu amene timapeza cifukwa comvela malamulo a Yehova , timayamba kukonda na kuyamikila kwambili Yehova na malamulo ake . M’nkhanizi , tidzaphunzila maumboni atatu amene akhala akudziŵikitsa anthu oimilako Mulungu . 9 - 10 . Ciwiya cina cikaonongeka , ndimagulilako kacipangizo kakale ndi kupeza wina wondikonzela . ” Ngati wina watilakwila , ndipo wapempha cikhululukilo , cikondi cimatilimbikitsa kuti tim’khululukile . Ndiye cifukwa cake pamene anaona mwana waoyo akubwela “ capatali ndithu , ” io anamuthamangila ndi kumulandila . Pofotokoza mmene tingayandikilile Mulungu , mau oyamba m’buku lakuti Yandikirani kwa Yehova amati : “ Pa ubwenzi uliwonse umene timapanga , timagwilizana ndi munthuyo cifukwa cakuti timamudziŵa , ndiponso kuti ali ndi khalidwe lapadela limene timalisilila ndi kuliona kukhala labwino zedi . Mogwilizana na mau amenewa , mu ulamulilo wa Solomo , mwana wa Davide , mtundu wa Aisiraeli unali pa mtendele na ulemelelo wosaneneka . Iye anali kukhala patsinde pa mtengo wa kanjedza ndipo anali kutumikila anthu malinga ndi zigamulo zocokela kwa Yehova . Conco musaope kapena kucita mantha . ” — Deut . Cifukwa tikukhala m’nthawi ya kukhalapo kwa Kristu . Joachim anayankha kuti : “ Ndinali wokhumudwa ndi wonyada . Ziyeneletso zimenezi zidzatithandiza kukumbukila nchito yaikulu imene akulu amacita mumpingo , ndipo tidzayamba kuwalemekeza kwambili . Imatithandizanso kudziŵa mmene tingatetezele zikhulupililo zathu . — Ŵelengani 1 Petulo 3 : 15 . Koma pambuyo pomenyedwa kwa masiku 10 , komanso cifukwa comuwopseza kuti adzacitila zaciwawa banja lake kudziko limene anacokela , anam’kakamiza kuyamba uhule . Zimenezi zikadzacitika , imfa idzaonongedwa kothelatu . Panthawiyo , iwo anali na mwayi wapadela wothandiza kukwanilitsa colinga ca Yehova , ndipo akanatelo , akanadalitsidwa . Ngati tafufuza pankhani imeneyi , tikhoza kuona kuti Ezekieli analemba mau amenewa pafupifupi zaka 612 Kristu asanabwele . ( b ) Timaonetsa bwanji kuti tikucilikiza Ufumu wa Mulungu masiku ano ? Mu September 1919 , dziko la France ndi la Poland linasainilana cikalata colola anthu a ku Poland kusamukila ku France . 14 - 16 . ( a ) N’cifukwa ciani n’kofunika kuuza mwininyumba colinga cimene tabwelela ? Anapempha kuti Abulahamu athamangitse Hagara na Isimaeli . — Genesis 21 : 8 - 10 ; Agalatiya 4 : 22 , 23 , 29 . Zoona n’zakuti Mulungu analenga anthu na makhalidwe apadela amenewa kuti azisangalala na moyo kwamuyaya pano padziko lapansi . Mungacite bwanji ngati muona kuti simungafotokoze bwino - bwino za cisanduliko kapena cilengedwe ? Ndinamenya nkhondo yandekha kuti ndithetse kupanda cilungamo ndi nkhanza ( A . Iye azidzayankha kuti , ‘ Zilonda zimenezi zinabwela cifukwa comenyedwa m’nyumba ya anthu amene anali kundikonda kwambili . ’ ” Pambuyo pofunsila kwa dokota amene anali kuwathandiza , Thierry ndi Nadia anapempha amayiwo kuti abwele kudzakhala nawo ku Madagascar . ( Genesis 1 : 28 ) Anali na mwayi waukulu wosamalila na kukulitsa malile a Paradaiso zungulile dziko lonse ! N’NABADWA mu 1926 , m’mudzi waung’ono wochedwa Karítsa , m’dziko la Greece . 11 : 1 - 5 . ( Ŵelengani Afilipi 2 : 3 , 4 . ) Muzifufuza . Tamandani Kristu , Mfumu Yaulemelelo , 2 / 1 Pamene mtumwi Petulo anali m’ndende , mngelo anaonekela kwa iye na kum’cotsa m’ndendemo . — Machitidwe 12 : 1 - 11 . ( 1 Pet . 2 : 2 ) Mwacitsanzo , kusinkha - sinkha coonadi ca Mau a Mulungu kunathandiza Yesu kuti asagonje atakumana ndi ciyeso . Nafenso ngati titsatila mfundo za m’Baibo , tidzatha kupewa mzimu wokonda cuma . ( Mat . Anacita zimenezo kuti apeleke “ dipo kuwombola anthu ambili . ” ( Afil . 2 : 5 - 8 ; Mat . Yesu anali ‘ Mwana wa mbewu ya Davide monga mwa thupi . ’ ( Aroma 1 : 3 , Buku Lopatulika . ) Cilengezo cakuti M’bale Pierce waikidwa kukhala membala wa Bungwe Lolamulila cinapelekedwa pa October 2 , 1999 , pamsonkhano wa pachaka wa Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania . 32 Mlongoza Nkhani wa Nsanja ya Mlonda 2017 Pa nthawiyo , mpingo wa kwathu wa Mboni za Yehova n’nali kuuona monga kilabu ya nkhalamba . Kodi anthu ambili othaŵa kwawo amakumana ndi mavuto otani asanacoke m’dziko lawo komanso pothaŵa ? Monga taonela , Paulo anapeleka malangizo kwa Timoteyo ofotokoza mikhalidwe imene ingacititse kuti akazi amasiye acikristu alandile thandizo la mpingo . N’ciani cingacitike ngati tiika maganizo athu onse pa zofuna zathu ? Tingaonjezelenso utumiki wathu pa nyengo imeneyi . Malinga ni 2 Timoteyo 1 : 7 , ndani maka - maka amene angatithandize kukhala olimba mtima ? Kukhala na mtima wodzimana waconco pofuna kuika zinthu za Ufumu patsogolo , ni umboni wakuti timaona ubwenzi wathu na Mulungu komanso cuma cauzimu , kukhala zofunika kwambili kuposa cuma cimene tingapeze m’dzikoli . Yehova anati : “ Mukhale oyela , cifukwa ine Yehova Mulungu wanu ndine woyela . ” ( Lev . 19 : 2 ; Deut . Kuti tikhale odzicepetsa , tiyenela kuziona moyenela . N’zoona kuti angakhale ndi imvi , koma mwina thanzi lao silofooka kwambili monga mmene Solomo anafotokozela . Mulungu amaticenjeza kudzela m’Mau ake ndi mumpingo kuti tiyenela kupewa zinthu zimene zingatigwetsele m’mayeselo . Zina mwa zinthu zimenezi ndi kuonongela nthawi yathu , ndalama zathu ndi mphamvu zathu pa zinthu zosathandiza kwenikweni . Ndipo Baibo imanena kuti Yesu tsopano ali ndi “ makiyi a imfa . ” N’cifukwa cake anakamba kuti : “ Ndine woyela pa mlandu wa magazi a anthu onse . ” Kodi Yesu anali kulidziŵa bwanji Baibulo ? Ana amafuna kuti makolo ao azikhala bwino cifukwa amaŵakonda . Mwacitsanzo , ganizilani mmene zipembedzo zasoceletsela anthu mamiliyoni ambili kuti asadziŵe zoona ponena za Mulungu , Baibo , tsogolo la anthu , ndi zinthu zina zambili . ( Luka 12 : 15 ) N’cifukwa ninji Yesu anapeleka cenjezo lamphamvu limeneli ? Kodi maina akuti “ Satana , ” “ Mdyelekezi , ” “ njoka ” ndi “ cinjoka ” amatiuzanji za mdani wamkulu wa Yehova ? Tiyeni tikambilane citsanzo ca wophunzila wa Yesu , Timoteyo . — Mac . 16 : 1 - 3 . N’ciani cimene mwatsimikiza mtima kucita m’caka conse ca 2015 ? 12 N’CIFUKWA CIANI PALI MA BAIBO OSIYANA - SIYANA ? Mulungu anaumba Adamu “ kucokela kufumbi lapansi ” ndipo anali atamuuza kuti “ kufumbiko udzabwelela . ” M’bale Mumba : Zimenezi n’zoona . Iwo amakumana ndi mavuto ambili ndipo ambili amabwelako ali ndi nkhongole zazikulu . Amene ali m’cipembedzo ca zoona amakhala okondana ndi ogwilizana monga gulu la abale la padziko lonse . — 1 Petulo 2 : 17 Lemba limodzi limeneli , mwa mau ophiphilitsa , limaonetsa mmene Yehova adzacotsela mavuto onse amene anthu akumana nawo kuyambila mu Edeni . N’cifukwa ciani mphatso ya Mulungu ya dipo la Yesu ndiyo yoposa zonse zimene tingalandile ? ( Yes . 32 : 1 ) Ulamulilo wa Yesu udzabweletsa “ kumwamba kwatsopano ” ndi “ dziko lapansi latsopano ” mmene “ mudzakhala cilungamo . ” Iye anati cikondi “ cimakwilila zinthu zonse . ” Mayankho anu otsimikiza ndi omveka bwino , anaonetsa poyela kuti munadzipeleka na mtima wonse , ndi kuti munali oyenelela kubatizidwa monga mtumiki woikidwa wa Yehova . Koma ife tili na mwayi ngako cifukwa tadziŵa mmene tingalemekezela ena mogwilizana ndi malangizo a Yehova . Ndiyeno tingam’funse kuti , “ Kodi cikanakhala cilungamo kuuza Adamu kuti adzabwelela ku nthaka ngati iye anali kudzapitadi ku moto wa helo ? ” 16 : 5 ) Tiyenelanso kudzifufuza ndi kuona mmene timaonela anthu a mtundu wina , a dziko lina , kapena a cikhalidwe cina . * Ulendo wapita , munafunsa funso lokhudza Ufumu wa Mulungu . Anzake ndi amene akutsogolela podutsa m’madela amene Timoteyo akudziŵa bwino . Iye anali kuseŵenza pa kampani inayake yapamwamba , ndipo anali kulandila ndalama zambili . 10 - 12 . ( a ) Kodi Mkristu amene akusamalila wacibale amene ali ndi matenda aakulu angakumane ndi mavuto otani ? Iye anati : “ Nimaona kuti Yehova amanipatsa mphamvu na kunitsogolela nthawi zonse . ” Kuti mpingo upitilize kukhala woyela ndi wogwilizana , akulu afunika kusamalila nkhani zaciweluzo mwamsanga komanso mwacikondi . Vesi 12 “ Tsoka dziko lapansi ndi nyanja , cifukwa Mdyelekezi watsikila kwa inu , ndipo ali ndi mkwiyo waukulu podziŵa kuti wangotsala ndi kanthawi kocepa . ” Ngakhale kuti ndise opanda ungwilo , Yesu anatilandila . Nanga ise n’kulekelanji kulandila ena ? ( 1 Pet . 3 : 18 ) Yehova analandila nsembe ya munthu mmodzi wangwilo , Yesu , monga dipo , kapena mtengo wogulila banja la Adamu ndi kuwapatsa ciyembekezo ca moyo wosatha umene Adamu anataya . ( Mat . 22 : 37 - 40 ) Njila yaikulu imene timaonetsela kuti timakonda mnansi wathu , ni mwa kumvela lamulo lakuti tizilalikila uthenga wabwino wokamba za Ufumu wa Mulungu . Mulungu anacita pangano ndi Aisiraeli a kuuzimu . Lamulo lakuti akulu ansembe aciisiraeli azikhala oyela mwakuthupi , lili ndi tanthauzo lalikulu kwa anthu a Yehova masiku ano . Mau ake amatilangiza kuti tiyenela kumutamanda , kum’patsa ulemu , ndi kumumvela . Kumbukilani kuti cifukwa ca mtima wofuna kuchuka na kulamulila ena , Satana anapandukila Mulungu . Koma kodi palipano iye ali na cimwemwe ? Kutalitali ! Ali na mkwiyo . ( Mat . Mofananamo , ngakhale kuti pali pano sitingathetse kupanda ungwilo kwathu ndi mtima wodzikonda , tifunika kuzindikila makhalidwe amene angayambitse mtima wodzikonda ndi kuyetsetsa kuwapewa . ( 1 Akor . Monga Davide , tili ndi cidalilo cakuti iye sadzatisiya tikadwala . Moyo umakhala wopanda phindu ngati munthu amangoika maganizo ake pa zinthu zimene angakhale nazo panopa . Yehova anamvela cifundo anthu ake Aisiraeli ngakhale pamene anali kum’cimwila . 11 : 2 ) Mfumu Yesu Kristu , amene ndi Mkwati amaona kuti mkwatibwi wake ndi “ wokongola ” mwakuuzimu . Zikusonyeza kuti Mdyelekezi salemekeza moyo wa munthu . Koma ndimasinkhasinkha malemba aŵili amene amandilimbikitsa . M’kupita kwa nthawi iwo anafa , monga mmene Mulungu anawacenjezela . Motelo , abale sam’kaikila kuti ndi woyenelela kukhala woyang’anila , ndi kuti angawathandize akakhala ndi mavuto . 24 : 5 , 6 ) Milandu yabodza imeneyi ikanacititsa kuti Paulo aphedwe . Koma pambuyo pophunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova kwa miyezi iŵili , ndinatsimikizila kuti Baibulo ndi loona . Ndiyeno Yesu anati : “ Amene ayeletsedwa si anthu 10 kodi ? Cilungamo ca Mulungu cidzabweletsa mtendele na citetezo padziko lapansi . — Yesaya 32 : 16 - 18 . Ndi maphunzilo otani amene Mose anaona kuti ndi apamwamba ? Kwa zaka zambili , iwo anali kuganizila zowonjezela utumiki wawo mwa kukatumikila ku dziko lina , koma Perrine anali kuopa . N’cifukwa ciani kutsutsa ulamulilo wa Mulungu n’kusaseŵenzetsa bwino ufulu wosankha ? Ngati muli ndi atumiki a pa Beteli mumpingo wanu kapena m’dela lanu , mungacitenji kuti muwathandize ? Inde , tisaiŵale kuti Yehova amatifunila zabwino . 22 : 34 - 40 ) Motelo , mudzapezekepo pa Mgonelo wa Ambuye . ( a ) N’ciani cinathandiza Yosefe kukana ciyeso ? Izi zitanthauza kuti muyenela kuika zolinga zauzimu patsogolo mu umoyo wanu . N’cifukwa ciani Mose anacita mantha ? Ciyeso cina cimene tifunika kupewa ndi kuonelela zamalisece . Kucita zimenezo kulibe vuto lililonse . * Iye anagaŵila akapolo ake cuma cake asanapite ku dziko lakutali , ndipo anali kuyembekezela kuti akapolo onse adzagwilitsila nchito cumaco kucita malonda iye akali ku dziko lakutali . Komanso , mungadziŵe mocitila ndi mavuto obwela cifukwa ca kupanda ungwilo . Ngakhale kuti nthawi zambili n’nali kupita nekha mu ulaliki , n’naphunzilanso zinthu zina cifukwa colalikila ndi ena . Ngati cifundo cimene tili naco pa anthu amene timawalalikila cayamba kucepa , cangu na luso lathu mu ulaliki zimayambanso kucepa . 1 : 22 ) Conco , anthu a mumpingowo anali na mwayi wotengela citsanzo ca Yesu ndi Atate wake mwa kukhululukila Petulo . Timapatsa anthu zinthu zimenezi popanda kulipilitsa . Mwamuna wina wokwatila ku Japan anati : “ Ndinali ndi vuto la zacuma . Patapita caka cimodzi , mkulu wanga Ilias , analoledwa kubwelela kunyumba kuti akasamalile amayi cifukwa atate anali atamwalila . Cikondi cimene tikamba ni capamwamba kwambili ndipo cimapangitsa munthu kukomela mtima ena , na kuika patsogolo zofuna za ena . ( Ezekieli 8 : 6 - 12 ; 9 : 2 , 3 ) Munthu ameneyo anauzidwa kuti apite mumzinda ‘ kukalemba cizindikilo pamphumi za anthu amene anali kuusa moyo ndi kubuula cifukwa ca zonyansa zonse zimene zinali kucitika mumzindawo . ’ N’cifukwa ciani Paulo anawauza mosapita m’mbali ? Cineneloci cinali ndi mau ambili ndi othandiza pofotokoza mfundo za coonadi . Iye anali atakwezedwa pa nchito yake yovina . M’malo mocita copeleka mwamseli , iwo ananama kuti apeleka ndalama zonse zimene anagulitsa munda , ndipo analangiwa cifukwa cocita zinthu mwacinyengo . Iye anati : “ Nthawi ina , mnzanga kunchito analemba meseji yoipa yokhudza khalidwe langa ndi kagwilidwe kanga ka nchito , n’kuitumiza kwa anzanga amene nimaseŵenza nawo . Tikamalalikila , timakhala tikugwila nchito mogwilizana ndi abale ndi alongo athu . Liphatikizapo zinthu zambili zimene anthu amaona kuti n’zofunika ngako pa umoyo wawo . Zinthu zimenezo zidzawonongedwa . Munthu amene amawayawaya kubatizika , akhoza kutaya mwayi wokalandila moyo wosatha . Cikhulupililo cake cinam’limbikitsa kuwalalikila molimba mtima , na kuwacenjeza za ciweluzo cimene Mulungu anali kubweletsa . Tikakhala pa misonkhano , tiyenela kumvetsela bwino - bwino ndi kulola zimene tiphunzila kukhudza mtima wathu . ( Yes . 35 : 5 , 6 ) Umphawi : Yehova adzauthetsa . ( Luka 22 : 32 , 54 - 62 ) Petulo anadzakhala mmodzi wa mizati ya mpingo wacikristu m’nthawi ya atumwi . Kodi Yesu sanakambe kuti “ aliyense wokhulupilila iye ” adzakhala ndi moyo wosatha ? ’ Nanga tingaonetse bwanji kuti timayamikila mwai wodziŵika ndi dzina la Mulungu loyela ? ( Yobu 42 : 3 ) Koma pambuyo poganizila cilengedwe codabwitsa ca Mulungu , Yobu ananena kuti : “ Ndinali kungomva za inu , koma tsopano diso langa lakuonani . ” — Yobu 42 : 5 . 5 : 16 , 22 , 23 ) Ngati mwapeza kuti maganizo anu akukhotelelabe ku zinthu zakuthupi ndi zilakolako za thupi , musalefuke . ( 2 ) Tiyenela kupita kukakambilana ndi m’bale wathu pamodzi ndi munthu wina amene akuidziŵa bwino nkhaniyo kapena amene angatithandize . Zinali zovuta kuti tizoloŵele umoyo watsopano cifukwa zinthu kumeneko zinali zosiyana poyelekeza ndi ku North America . Ndi zocitika ziti zimene Akristu adzakumana nazo posacedwapa ? Nanga tikambilana ciani m’nkhani ino ? Ku Sri Lanka Kwa zaka 2,000 , adani a Mulungu ayesa kuti alepheletse kulengezedwa kwa uthenga wabwino . Felisa : Ndinakulila m’banja lina losauka ku Spain . Ni njila ina iti imene tingalimbikitsile Akhristu amene akutumikila mokhulupilika ? Mneneli wacikulile Samueli sakanakwanitsa kuumiliza ana ake kuti akhalebe okhulupilika pa mfundo zolungama zimene anawaphunzitsa . ( 1 Sam . Haykanush ndi mwamuna wake anafotokozela banjalo kuti zimene amaphunzila m’Baibulo , n’zimene zinawathandiza kukhala oona mtima . ( Deut . 3 : 27 , 28 ) Apa Yoswa anali kudzapatsidwa udindo waukulu wotsogolela Aisiraeli ku Dziko Lolonjezedwa . Atate ŵake anali kumufuna mwamsanga . — 1 Samueli 16 : 12 . Akhristu ena acicepele aphunzilako citundu cina . Komabe , sapeleka malangizo a m’mutu mwao . ( 2 Tim . 2 : 19 ) Iye “ amadziŵa njila za olungama , ” komanso amawapulumutsa akakhala pa mayeselo . ” — Sal . 25 : 7 , 8 . “ Nditayang’ana , ndinaona hachi yakuda . KUKHULULUKA Olaf , wa ku Germany , anali kapolo wa fodya kwa zaka 16 . Iye anayamba kukoka pamene anali ndi zaka 12 . Kumatithandiza kuti pokamba kapena poimba , mau azituluka mwamphamvu . Timagwilitsila nchito mathilaki , masitima a pamadzi ndi a pa mtunda potumiza Mabaibulo komanso zofalitsa zina . Tiyeni tione mmene tingatengele citsanzo ca Yesu . Koma m’tsogolo moyo wamuyaya , kaya kumwamba kapena padziko lapansi . Imfa , Mdani Wotsilizila , Idzaonongedwa Kucokela pamenepo , anzangawo anazindikila kuti inenso nikali kulimbana na cizolowezi cimeneci ndipo analeka kunivutitsa . N’cifukwa ciani kumvela lamulo la Mulungu lokhudza magazi n’kofunika kwambili ? Ganizilani citsanzo ca Kathy . 72 : 13 - 16 ) Babulo Wamkulu sadzasoceletsanso aliyense , iye sadzakhalaponso . 13 : 23 ) Fanizo yoyamba ni ya mtengo wa mpesa . Kodi palinso cinenelo cofala kwambili masiku ano ? N’cinthu canzelu kufunsila na kumvela uphungu wa acikulile , aciyambakale . 11 : 24 . Ndiponso , dipo linapangitsa kuti zikhale zotheka kudzakhala kwamuyaya mwacimwemwe . Mitengo ya maolivi imeneyo inaimila “ odzozedwa aŵili , ” Bwanamkubwa Zerubabele ndi Mkulu wa Ansembe Yoswa , amene ‘ anaimilila kumbali iyi ndi mbali inayi ya Ambuye wa dziko lonse lapansi . ’ Popeza kuti anthu ambili analowetsedwa m’nkhondoyo , cidani cinafalikila m’maiko ambili . ” M’bale Franz anali na luso lomvetsela mwachelu nikamaŵelenga , ndiponso anali kukumbukila zinthu kwambili . Ngakhale atumiki a Mulungu aciyambakale amafunikila cilimbikitso . N’kutheka kuti cifukwa ca zimene Paulo anacita , Luka amene anali dokota komanso mnzake wa Paulo woyenda naye , anatsalila ku Filipi pamene Paulo na Sila anacoka . 13 : 4 , 5 . 10 , 11 . ( a ) Tizikhala na colinga canji pophunzila Mau a Mulungu ? Tonse timadwala . ( Yohane 16 : 23 ) Motelo , Yesu anatiphunzitsa kupemphela kwa Atate wake , amenenso ndi Atate wathu , Yehova Mulungu . — Yohane 20 : 17 . M’fanizo limeneli , pali nyengo ya nthawi kucokela pamene mau akuti “ Mkwati uja wafika ! ” Mwacitsanzo , Yesu anaukitsa mwana wa mkazi wamasiye kunja kwa mzinda wa Naini , na mwana wa Yairo ku nyumba kwawo . Izi zionetsa kuti mwina atumwi anafuna kuthetsa mikangano imene iyenela kuti inabuka pakati pa Akhiristu oyambilila . — Mac . 6 : 2 - 6 . Koma ambili amavutika kukhulupilila zimenezi . Okwatilana angalimbitse ukwati wao ngati amaika zofuna za mnzao wa muukwati patsogolo pa zao . ( Afil . Yehova analamula akulu a mu Isiraeli kuti aziweluza milandu mogwilizana na cilungamo cake . Iye anakamba kuti ndi wosangalala kwambili kuti anasankha kubatizidwa . John ndi Melvin Zioneka kuti patapita nthawi , okopa Baibo anacotsamo dzina la Mulungu na kuikamo dzina la Cigiriki lakuti Kyʹri·os , lotanthauza kuti “ Ambuye . ” Mulimonse mmene zinthu zingakhalile kwa ife , tiyeni tiike patsogolo zinthu za Ufumu wa Yehova . Amenewa ndi mau olondola ndiponso omveka bwino . Munthu amene amakwiya msanga sangakhale na banja lacimwemwe . Koma akamaliza nchito yake , amaweluka ndi kupita kunyumba kukakhala ndi banja lake ndi kucita zinthu za kuuzimu . Buku lina lofotokoza Baibo linakamba kuti munthu wodzikonda ali ngati “ kanyama kochedwa kanungu [ kapena kuti kansoni ] , kamene . . . kamadzipinda n’kukhala ngati bola . Kamamva kuthuma bwino pobisa mutu na miyendo yake , . . . koma . . . kwa ena kamaonetsa minga zokha - zokha . ” Yesu anali kuzindikila zimene Yehova anali kufuna kuti iye acite . Kuposa zonse , timakondweletsa Atate wathu wakumwamba , Yehova . Kaŵili - kaŵili nimamvela ngati mmene Yesu anamvelela pamene anapempha Atate wake kuti , ngati n’kotheka alole mavuto kumupitilila . 9 : 2 . ) Ngakhale patapita zaka 70 ali ku Babulo , anali kudziŵikabe na dzina la Ciheberi . — Dan . Pogwilitsila nchito makhadi a ulaliki , kodi panali mavuto otani ? M’nkhani ino , tiphunzila mmene Yehova amakambila ndi anthu m’njila yosavuta . Kodi Antonio anacita ciani ? ( b ) Tiyenela kumva bwanji ena akamatizunza pokhala Mboni za Yehova ? Khalanibe na ciyembekezo . Padziko lapansi , anthu a Mulungu adzaoneka ngati alibe citetezo ciliconse . Iye anati : “ Pamene ndinakhala cete osaulula macimo anga , mafupa anga anafooka , cifukwa tsiku lonse ndinali kuvutika mumtima mwanga . Anthu okopela ndi omasulila malemba anayesa kusintha uthenga wa m’Baibulo . N’cifukwa ciani kukambilana zimenezi n’kofunika ? Pangano la Cilamulo linayamba kugwila nchito pa Phili la Sinai mu 1513 B.C.E . Mwacitsanzo , Christine anali na zaka 10 pamene anadziikila colinga cakuti nthawi zonse aziŵelenga nkhani zofotokoza mbili ya Mboni za Yehova zokhulupilika . Zimenezi zinacitika mu October 1914 , ndipo cinali ciyambi ca “ masiku otsiliza ” a dongosolo loipa la Satana . — 2 Tim . Asanapite pa ulendo , mbuyeyo anapatsa akapolo ake ndalama ndi kuwauza kuti amuculukitsile ndalamazo . Atabwelako ku ulendo wake , iye anaŵelengelana ndi akopolo ake ndi kuona mmene anagwilitsila nchito ndalamazo . ( Mat . Mwacidule tinganene kuti , ana acikulile acikristu ndi amene ali ndi udindo wosamalila zosoŵa za makolo ao . Zipatala zinali zocepa . Conco , anthu ambili odwala anali kusamalidwa kunyumba ndi acibale awo , ndipo anali kumwalilila m’nyumba . Iwo amagwilitsila nchito mpatuko , citsutso , anthu aciwawa , ziletso , cizunzo , ndi kupha . NKHANI YA PACIKUTO | BAIBULO — MMENE YAPULUMUKILA Iye sanacite nsanje pamene Davide anadzozedwa kuti adzakhale mfumu ya Isiraeli yotsatila . Iye ali pafupi ndi onse amene amamuitana m’coonadi , ndipo anthu amene amamuopa adzawacitila zokhumba zawo , adzamva kufuula kwawo kopempha thandizo ndipo adzawapulumutsa . ” 16 , 17 . Anthu ambili ku Yuda anali na makhalidwe oipa pa nthawi imene Danieli anali wacicepele . ( 2 Mbiri 20 : 7 , Buku Lopatulika ; Yesaya 41 : 8 ; Yakobo 2 : 23 ) Ndiye yekha amene amachulidwa mwacindunji m’Baibulo kuti anali bwenzi la Mulungu . * Ngakhale kuti akuluwo ndi ocokela m’maiko osiyanasiyana , malangizo amene anapeleka ndi ofanana kwambili . Conco , nthawi zina tingakhumudwe na mau kapena zocita za Mkhristu mnzathu , kapena ise tingakhumudwitse mnzathu . Magaziniyi ya Nsanja ya Mlonda idzatithandiza kudziŵa mphatso imodzi yoposa zonse , yocokela kwa Mulungu . Akristu oyambilila naonso anali kucita zinthu mogwilizana . VENECIA , mlongo wa ku Venezuela , anati : “ N’nali kuganiza kuti siningakwanitse ulaliki wa pa foni . ” Asanayambe nchito yomasulila Baibo , Lefèvre anali kuphunzila mozama mabuku a ziphunzitso za anthu ndi a zacipembedzo kuti amvetsetse zimene zinalembedwa . Pokamba za mwamunayo , Baibo imati : “ Kenako anapita kukabatizidwa . ” ( Mac . ( Mat . 12 : 34 ) Ngati mwaona kuti zocita za anzanu zikuika ubwenzi wanu na Yehova paciopsezo , citamponi kanthu mofulumila mwa kupewa kugwilizana nawo kwambili kapena kungothetsa ubwenziwo . — Miy . Nthawi zina tinali kukomboka 23 : 00hrs usiku . Koma usadye zipatso za mtengo wodziwitsa cabwino ndi coipa . Cifukwa tsiku limene udzadya , udzafa ndithu . ’ ” — Genesis 2 : 15 - 17 . Ganizilani zimene mkulu wina , amene watumikila kwa zaka zambili , wakhala akucita . Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Sitikucita ciliconse cokhumudwitsa , kuti utumiki wathu usapezedwe cifukwa . ” Njala , zivomezi , milili ndi kukwanilitsidwa kwa maulosi ena a m’Baibo ndi umboni wamphamvu wosonyeza kuti Yesu Kristu anayamba kulamulila kumwamba monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu mu 1914 . Amaganizila za tsogolo lathu ndipo afuna kuti tikakhale ndi umoyo wabwino kwambili . Pamene anafuna kum’kwapula , anafotokoza kuti anali nzika ya Roma . Ine na Maria , tinali kukondwela tikapita kukaceza kumalo kumene ana athu anali kutumikila . Conco , pitilizani kuŵelenga Baibo tsiku lililonse , na kupezeka ku misonkhano ya mpingo nthawi zonse . Mau ake ni akuti : “ Esibaala Beni [ mwana wa ] Beda ’ . ” Komabe , anali odula kuwilikiza ka 10,000 pamtengo wake weniweni . Iye ananena kuti : “ Apolisi mofuula anati : ‘ Tidzatsimikiza kuti palibe adzakumbukanso dzina la Yehova mu Estonia ! Kodi mpingo unafunikila kucita naye bwanji munthu wa conco ? 1 : 2 ; Aroma 12 : 12 ) Cikondi cathu pa Yehova cidzatisonkhezela kucita zinthu zomukondweletsa nthawi zonse . Lembali limati : “ Cifukwa kukonda Mulungu kumatanthauza kusunga malamulo ake , ndipo malamulo akewo ndi osalemetsa . ” Kodi izi zikanacitika ngati Yesu sanaukitsidwe kwa akufa ? Nkhani ya Petulo pamene anayenda pa Nyanja ya Galileya ingatiphunzitse zinthu zofunika pankhani ya cikhulupililo . Njila ina imene tingakumbukile Bungwe Lolamulila ndi mwa kudzipeleka pa nchito yolalikila . Imfa ya Yesu Kristu ndi kuukitsidwa kwake zinatimasula ku ukapolo woipitsitsa kupambana wina uliwonse , ukapolo ku ucimo ndi imfa . Kodi malemba a 1 Akorinto 10 : 31 ndi Afilipi 2 : 4 , angatithandize bwanji pankhani ya mavalidwe ? N’nadziŵa kuti mnzangayo kapena Yehova sindiwo anacititsa mavuto amene n’nali kukumana nawo . Pofika cakumapeto kwa zaka za m’ma 1920 , kagulu kocepa ka Ophunzila Baibo * ku Australia kanali katalalikila kwambili m’mizinda ya m’mbali mwa nyanja , m’matauni , ndi m’madela ena ozungulila . Timawakonda ndi kuwaganizila ndipo sitifuna kuwakhumudwitsa ndi mau athu Zimenezo zinakwanilitsanso ulosi wa m’Baibo wakuti Mesiya adzaikiwa m’manda “ limodzi ndi anthu olemela . ” — Yes . Kodi nkhondo yafika pamlingo wotani masiku ano ? Mbuye anakamba kuti kapoloyo anali “ woipa ndi waulesi . ” Kodi Mulungu anatipatsa mphatso yotani imene imatithandiza kukhala ndi cikhulupililo ? Anali kudya na kumwa . 7 : ​ 1 - 4 ) Cidindo cimeneco cidzakhala umboni wakuti adzapitadi kumwamba . Nkhani yoyamba idzafotokoza mmene tingatulile Mulungu nkhawa zathu . Conco , Yesu anawauza kuti : “ Ufumu wa Mulungu udzacotsedwa kwa inu n’kupelekedwa kwa mtundu wobala zipatso zake . ” — Mat . Ndipo anacita zinthu zina zabwino posamalila anthu a Yehova . ( Mat . 25 : ​ 5 , 6 ; 26 : 41 ) Mofananamo , Akristu odzozedwa okhulupilika m’masiku otsiliza ano alabadila mau akuti “ Mkwati uja wafika ! ” Iye anapempha malo obisalako kwa Yaeli , mkazi wa Hiberi Mkeni , ndipo anamulandila . Koma sitinali kudziŵa kuti tingapite kuti . Titaŵelenga nkhani yokhudza dziko la Myanmar ya mu Buku Lapachaka la 2013 , tinakhudzidwa mtima na zocitika zolimbikitsa zimene tinamva cakuti tinayamba kuganizila zokatumikila m’dzikolo . ” Yelekezelani kuti mukumva wacicepele ameneyu akuuza Goliyati kuti : “ Iwe ukubwela kwa ine ndi lupanga , mkondo ndi nthungo , koma ine ndikubwela kwa iwe m’dzina la Yehova wa makamu , Mulungu wa asilikali a Isiraeli , amene iweyo wam’tonza . ” “ Mayiyo anacita mantha ndi kuyamba kunjenjemela , ndipo . . . anafika pafupi n’kugwada pamaso pake ndi kumuuza zoona zonse . ” Mufunikanso kuganizila zimene Aminoni anacita , ndi mavuto amene anakumana nawo cifukwa ca khalidwe lake loipa . A Zulu : Inde . Kodi anthu ambili apindula bwanji ndi Baibulo la Dziko Latsopano ? Iye anapempha Yehova kuti amuthandize kusankha mkazi amene Isaki anafunika kukwatila . Cilamulo cimeneco ciphatikizapo zonse zimene Yesu anaphunzitsa . UBWINO ( a ) N’cifukwa ciani Yehova yekha ndiye ali na ufulu wocita ciliconse ? M’Dziko Lolonjezedwa , Aisiraeli anali kupatsidwa colowa malinga ndi kuculuka kwa anthu . 4 : 6 , 7 ) Komabe , mau a Yehova amenewa alinso na tanthauzo lalikulu lokhudza zimene zikucitika masiku athu ano . Claudia anakambanso kuti : “ Zilibe kanthu kaya uli pabanja kapena ayi , ukhoza kukhala wosangalala ngati upatsa Yehova Mulungu zinthu zabwino koposa . ” — Salimo 119 : 1 , 2 . Koma anasintha . Akhristu afunika kukhala na maganizo oyenela pankhani yopeleka ulemu . ( b ) Ni mafunso ofunika ati amene tidzakambilana tsopano ? N’cimodzimodzinso ndi anzake atatu a Danieli . Iwo anapatsidwanso maudindo . — Dan . NKHANI YA PACIKUTO | BOMA LOPANDA ZIPHUPHU Abigail , mtsikana wa zaka 18 , anati : “ Nthawi zina , kukamba zoona kungaoneke monga kosathandiza , maka - maka ngati zioneka kuti kunama kungakupulumutse ku mavuto . ” Mmodzi wa abale anga anayamba kulambila Yehova , ndipo amai naonso mpaka nthawi imene anamwalila , anali kukamba zabwino za cipembedzo cathu akamaceza ndi ena . Kodi Yehova amawaphunzitsa bwanji anthu ake kukhala acifundo ? Kodi munthu wakuthupi tingam’dziŵe bwanji ? N’cifukwa ciani kukhala woceleza , woolowa manja , wokhululuka , ndi wokoma mtima kwa Akhristu anzathu n’kofunika kwambili ? Anthu ambili andale na ena amakonda kucita zionetselo za kusakondwa , kuukila boma , na kucita makampeni ofuna kusintha zinthu m’dziko . Dzifunseni kuti : ‘ Kodi anthu a m’dela langa amaniona bwanji ? Nkhaniyi si yopeka , inacitikadi . Kodi munakwanitsa kusankha zinthu moyenela ? Ngati watiuza kuti ndi wotangwanika , tingam’pemphe kuti tilankhule naye mwacidule , ndipo tiyenela kucita zimenezo . Gulu laciŵili limeneli ndi anthu amene akuyembekezela kudzakhala padziko lapansi . Mwina zimenezi zinacitika pamene munaona koyamba dzina la Mulungu lakuti Yehova m’Baibulo . 24 : 15 ) Kodi tingakambe kuti io “ ayesedwa oyenelela ” kudzaukitsidwa ? Kumasuka kwa Blessing mu ukapolo nakonso ni kodabwitsa . ( a ) Kodi zinacitika bwanji kuti ena apanduke m’banja la Mulungu ? “ Samalani : mwina wina angakugwileni ngati nyama , mwa nzelu za anthu ndi cinyengo copanda pake , . . . [ ca ] m’dzikoli . ” — AKOL . ( Yohane 2 : 25 ) Yesu anali kudziŵa zimene zinali m’mitima yao . Iwo sapatsidwa ulemu mmene Mulungu amafunila . CIFUNDO , KUKHULULUKA Tatumikila pamodzi mosangalala monga banja kwa zaka 51 . N’nali kuona kuti anthu amene amalalikila si amuna eni - eni . Cikondi cimeneci cimam’limbikitsa kucita ciliconse cimene wafuna . Buku lina lakuti Jesus and His World linati : “ Ubweya unali kupezeka m’mitundu yosinasiyana , wina unali woyela , wina wofiilila wooneka ngati wakuda . ” Asilikali a Koresi anagwilitsila nchito njila yaluso popatutsa madzi a mtsinje wodutsa mumzinda wa Babulo ndipo mtsinjewo unauma . 3 : 5 ) Kodi zimene Adamu na Hava anasankha kucita zinawaonjezela ufulu ? Iye anatsimikiza mtima kusintha umoyo wake . Conco , analoŵa nchito ndi kupempha abwana ake akale kuti amucepetseleko malipilo a pamwezi obweza nkhongole . Izi zidzacititsa kuti anthu omvela adzakhale ndi moyo wabwino kwamuyaya . Koma kaamba koŵelenga Baibo , naphunzila kukhala wodziletsa . Lembani bajeti imene mudzakwanitsa kuitsatila . Ndiponso io sadzafanso , cifukwa adzakhala ngati angelo . Iwo adzakhalanso ana a Mulungu mwa kukhala ana a kuuka kwa akufa . ” — Luka 20 : 34 - 36 . Popeza tinali kugwila nchito yapamwamba , tinali kugula zakudya m’malestilanti apamwamba , kuyenda ku mayiko ena , ndi kugula zovala zodula . Mwacitsanzo : Tinene kuti mwana wanu wamng’ono wakupemphani kuti mum’gulile njinga , kodi mungam’gulile nthawi imeneyo ? Mwacitsanzo , Yesu anakambilatu kuti m’masiku otsiliza , ophunzila ake adzalalikila uthenga wabwino wokamba za Ufumu wa Mulungu padziko lonse lapansi . Poona zitsanzo za anthu okhulupilika akale , tidzaona mmene tingaikile cidalilo mwa Yehova kuti adzaticilikiza pocita zimene tingathe polimbana ndi mavuto athu ndi kuthandiza ena . N’cifukwa ciani kudzikonda pa mlingo woyenelela kuli cabe bwino kwa Mkhristu ? Zotulukapo za ukapolo umenewu n’zakuti timakhala na nkhawa , timavutika , ndipo pamapeto pake timafa . Kuonjezela pa zimene mumaŵelenga m’Baibulo , pali zinthu zina zimene mungasinkhesinkhe . Iye analibe nthawi yokwanila yosonkhana ndi yolalikila . Ndipo anafunika kugonjetsa ciyeso cocokela kwa abwana ake cakuti agone naye . Mwacitsanzo , Mulungu anacititsa Nowa kukhala womanga cingalawa , anacititsa Bezaleli kukhala mmisili waluso , anacititsa Gidiyoni kukhala wolimba mtima pa nkhondo , ndipo anacititsa Paulo kukhala m’mishonale . Ngakhale masiku ano , abale ku Mexico amakonda kwambili zinthu zauzimu . — Za m’khokwe yathu ku Central America . Coyamba , tiyeni tikambilane mau akewo , amene apezeka pa Afilipi 4 : 6 , 7 . ( b ) Fotokozani cocika ca banja lina limene linaonetsa cikhulupililo colimba . Zinatheka bwanji kuti tikhaleko ? Kodi fanizo la Yesu la mwana woloŵelela limatanthauza ciani ? Ine naona kuti ngati munthu ali na mtima wofuna kutumikila , Yehova amam’dalitsa . Pamene tiganizila kwambili cifukwa cimene tiyenela kukondela anzathu , ndi bwino kukumbukila mau a Yesu akuti , Atate wake “ amawalitsila dzuwa lake pa anthu oipa ndi abwino , ndi kuvumbitsila mvula anthu olungama ndi osalungama omwe . ” N’zoona , pokhala anthu opanda ungwilo , tonse timalakwa . Baibo inakambilatu momveka bwino zimenezi . — Genesis 1 : 1 . Ngati sitisamala tingayambe kuganiza kuti mbali zina za m’Baibulo kapena zofalitsa zina sizitikhudza . Mariya anabeleka Yesu . ( Mat . 23 : 12 ) Ngati tili na mtima wodzicepetsa , ndiye kuti tidzapewa kutengela mzimu wodzikweza wa anthu a m’dzikoli . Ndipotu osati uthenga wokha ayi , komanso miyoyo yathu yeni - yeniyo , cifukwa tinakukondani kwambili . ” — 1 Ates . Baibo imati : Malinga ni mau a Yesu , kodi alembi na Afarisi anaonetsa bwanji kuti sanali kulemekeza moyo ? Ogwila nchito ku mafamu nthawi na nthawi anali kupatsidwa cakudya , koma anali kulandila malipilo awo kamodzi pa caka . Mwacitsanzo , kulandiwa udindo kungam’thandize kuona kufunika kocita phunzilo la Baibo laumwini , kusinkha - sinkha , na kupemphela . Ngati mufuna kudzatumikila monga mkulu mtsogolo , muzigwila nchito mwakhama ndi kukhala wokhulupilika pa utumiki uliwonse wopatulika . Panali mamvekedwe a lipenga amene anali kusonyeza kuti anthu afunika kusonkhana pamodzi . Iye anati “ Wapolisi ananifunsa kumene timatenga zofalitsa zathu ndipo ine n’namuuza kuti timazitenga ku Brooklyn . Iye anali atayenda kwa milungu ingapo kulowela kumpoto ndipo anali kucokela ku Phili la Horebe limene linali kutali . Kuti akwanitse ciŵelengeco , ofalitsa anafunika kuthela maola 15 pa mwezi , ndipo apainiya maola 110 . Pamene Ababulo anaononga Yerusalemu mu 607 B.C.E . , amuna , akazi , ndi ana ambili anaphedwa . Kusintha kapumidwe . 24 : 3 , 12 ) M’zaka 100 zoyambilila , Ayuda amene anali kudzicha anthu a Mulungu , analola cikondi cawo pa Mulungu kuzilala . ndi imeneyo . Ulosiwo ndinauŵelenga mobwelezabweleza . wodzicepetsa ? Zikakhala conco , kodi tizikhala na kaonedwe kotani pokumana ndi citsutso ca m’banja ? 1 : 11 ) Zilizonse zimene Mulungu amacita zimapindulitsa ena . ( 1 Akor . 15 : 22 - 26 ) Ndithudi , imfa imene tinalandila kwa Adamu idzaonongedwa . Tiyenela kutsimikiza mtima kucita ciani ? Pa malonjezo amene takambilana , kodi inu munapangapo malonjezo angati kwa Mulungu ? Anthu ena amene tikuyesa kuthandiza angasiye Yehova . N’zoona kuti m’nyengo yotentha kungakhale kovutilapo kuvala zovala zina zaulemu . Malimba a m’nyimbo amakondweletsa . Enanso angafunike kusinkhukilapo kuti ayenelele ubatizo . Kuwonjezela apo , Nowa anadziŵa kuti nchitoyo idzacititsa kuti anthu azimunyoza kwambili na kumutsutsa . Salimo 37 : 9 imati : “ Oyembekezela Yehova ndi amene adzalandile dziko lapansi . ” Nsanja ya Mlonda iyi ifotokoza ena mwa malangizo othandiza opezeka m’Baibo , ndipo ikambanso zimene mungacite kuti mupindule na zimene mumaŵelenga m’Baibo . Onani mmene anatsatilila mfundo zimenezi pomasulila ma Baibo aŵili oyambilila . Mwina iye anali bize kusoka kacigamba pa tenti imene inali nyumba yawo . Zinthu zonse zimene zipangitsa anthu kuvutika kwambili zidzasila . Akatswili ofufuza zinthu amakhulupilila kuti zomela izi za mtundu wa maudzu zakhalako zaka masauzande ambili 14 Baibo na Tsogolo Lanu Mufunika kutambasula dzanja na kuilandila . ( Ŵelengani Aroma 15 : 7 . ) “ Pitilizani kuzindikila cifunilo ca Yehova . ” — AEFESO 5 : 17 . Motelo , mosataya nthawi ndinaganiza zoyamba upainiya . N’zoona kuti masiku ano , Akristu sangakwatile mitala , koma pakati pao pamapezeka mabanja ogaŵanika , makolo opeza , ana opeza ndi ang’ono kapena akulu athu opeza . ( 2 Timoteyo 3 : 1 ) Ulosi wa m’Baibo komanso zimene zicitika masiku ano , zionetsa kuti tili mu “ masiku otsiliza . ” Iwo angayambe kusamvetsetsa , kusaona bwino , kuiŵala - iŵala , ndi kuvutika kupita ku cimbudzi . 17 : 11 - 15 , 17 , 18 . Pokhala wacinyamata , kodi mumakonda kukhala ndi acinyamata anzanu ? Koma kodi Aisiraeli anacita ciani patapita nthawi ? Poyamba Yesu sanamuyankhe ciliconse . 27 : 62 - 66 . N’zoona kuti kukhulupilila n’kofunika . Mlongo wina wochedwa Vicky anati : “ Kwa zaka zingapo ndinasungidwa ndi ambuye , koma mng’ono wanga anali kukhala ndi makolo anga . Komanso , amalemekeza ufulu wathu wodzisankhila zocita . N’ciani cingatithandize kuti ulaliki wathu uzikhala wogwila mtima ? ( 1 Ates . 1 : 3 ) Yehova nayenso amakumbukila nchito zacikondi za aja amene amamutumikila mokhulupilika , kaya acite zambili kapena zocepa . — Aheb . Tingacite ciani kuti kusinkha - sinkha kwathu kuzikhala kwaphindu ? Sitingapeweletu kukhumudwitsa ena cifukwa ndife opanda ungwilo . Mwana wao akalakwa , amadzifunsa kuti : ‘ Kodi ndi nthawi yoyamba iye kucita zimenezi kapena cangokhala cizoloŵezi cake coipa ? ( Yobu 38 : 1 , 4 ) Conco , tonse tifunika kuona umboni na kuseŵenzetsa luso lathu la kulingalila kuti tidziŵe zeni - zeni . Komanso , kulimbikila nchito kumabweletsa madalitso . ( Miy . Yehova amaona kuti anthu akacitila zabwino atumiki ake , ndiye kuti acitila iyeyo . Sara anakulila mumzindawu umene anthu ake anali otangwanika kwambili , ndipo iye anali kudziŵana ndi anthu ambili . 7 : 5 , 16 . Kodi mukhulupilila kuti zimene imaphunzitsa n’zimene Khiristu anali kuphunzitsa , ndiponso n’zimene otsatila ake oyambilila anali kukhulupilila ? Chulan’koni khalidwe limodzi la umunthu watsopano . Banja lathu linali kukonda kwambili kulambila Yehova . Atate anali kulemekeza kwambili Baibo , ndipo izi zinacititsa kuti ifenso tiziyamikila Mau a Mulungu . Solomo anatama mtsikanayo kuti ndi “ wokongola ngati mwezi wathunthu , wosadetsedwa ngati dzuwa lowala . ” Cocitika cimeneco ndi kupulumuka cisautso cacikulu . Nthawi zambili , tikadziŵa cimene cipangitsa mavuto amene tikumana nawo , cimakhala copepukako kuwapilila . Iwo angakupatseni malangizo abwino ocokela m’Baibulo . Mofananamo , Yesu sanatanthauze kuti munthu aliyense amene adzaweluzidwa kuti ndi nkhosa ayenela kupatsa odzozedwa cakudya ndi zovala , kuwasamalila pamene adwala , kapena kupita kukawaona akakhala m’ndende . 17 : 7 ) Maina amenewa anali oyenelela cifukwa amatanthauza “ Kuyesa ” ndi “ Kukangana . ” ( Aroma 10 : 1 , 2 ) Kodi Paulo anafotokoza zifukwa ziti zimene anapitilizila kugwila nchito yake yolalikila ? Ulosi wocititsa cidwi kwambili ni wa pa Genesis 3 : 15 . Poyamba Aisiraeli anacita zinthu molimba mtima , koma patapita zaka 15 , anafooka . ( Hos . 14 : 4 ) Ha , n’citsanzo cabwino cotani nanga , coseŵenzetsa ufulu wake kupindulitsa ena ! ( Aefeso 4 : 31 , 32 ) Mwacitsanzo , anali kukwiya msanga . Komabe panthawiyo , Ayuda sanalinso pa ubwenzi wapadela na Yehova . M’dzikoli muli mipingo iŵili ndi magulu aŵili amene amagwilitsila nchito cinenelo ca Cibiribiri , ndipo muli mipingo itatu ndi magulu anai amene amagwilitsila nchito cinenelo ca Cikabeka . NYIMBO : 125 , 43 Kuona mmene Yehova anali kucitila zinthu ndi anthu Ake kunam’thandiza kudziŵa zinthu zimene Yehova amakonda ndi zimene amadana nazo . Ndiyeno , moleza mtima anawaongolela ndi kuwauza zimene anafunika kucita kuti asinthe maganizo ao . — Ŵelengani Yohane 6 : 25 - 27 . ( Mateyu 24 : 3 , 7 ; Luka 21 : 10 , 11 ; Chivumbulutso 6 : 3 - 8 ) Yesu anakambanso kuti : “ Cifukwa ca kuwonjezeka kwa kusamvela malamulo , cikondi ca anthu ambili cidzazilala . ” — Mateyu 24 : 12 . Mwacionekele , mau a Yesu amenewa anadabwitsa kwambili ophunzila ake . Popeza kuti Paulo anali nzika ya Roma , zimenezi zinakhudza mmene anthu a ku Filipi anayenela kucitila naye . ( Mac . Komabe , nkhani zake n’zogwilizana ndi zomveka bwino . Akacita zimenezi , amaonetsa kuti akulemekeza makonzedwe a Yehova okhudza umutu mumpingo wacikristu , cifukwa cakuti kuphunzitsa ndi udindo wa abale . ( 1 Akor . Openyelela seŵelo la “ Eureka ” anali kuyambila pa anthu ocepa mpaka m’mahandiledi . Malangizo a m’zofalitsa zimenezi , amawathandiza kulimbana ndi mavuto a kusukulu ndiponso amene amakumana nao pamene akukula . Malinga ndi Yohane 10 : 16 , Yesu anati : “ Ndili ndi nkhosa zina zimene sizili za khola ili , zimenezonso ndiyenela kuzibweletsa . Zidzamva mawu anga , ndipo zidzakhala gulu limodzi ndi m’busa mmodzi . ” 8 Dipo — ‘ Mphatso Yangwilo ’ Yocokela kwa Atate Ngati mai amene akulela yekha ana amabwela ndi ana ake kumisonkhano nthawi zonse , kodi simumayamikila cikhulupililo cake ndi kudzipeleka kwake ? Coyamba anamuongolela . Popeza ndise opanda ungwilo , nthawi zina zimativuta kukhala odziletsa . Kodi kukhala na ndalama komanso katundu wambili kumabweletsa cimwemwe cokhalitsa ? Mabanja angapo okhala m’dela lina ku Athens , m’dziko la Greece , akuphunzila nyimbo za Ufumu pa maceza acikhristu Nayenso Reylene wa ku Philippines anali na copinga cinacake . Mtumwi Paulo anatangwanika kwambili muutumiki wa Yehova pamene anali wacikulile . Caka cotsatila , m’bale Henschel anabwelanso ku Malawi kudzacititsa msonkhano wacigawo wapadela umene unacitikila kunja kwa mzinda wa Blantyre , ndipo anthu 10,000 anapezekapo . Munthu woyamba kuukitsidwa , anaukitsidwa na mneneli Eliya pamene Mulungu anam’patsa mphamvu yocita zozizwitsa . Kucita zimenezi ni cikondi , ndipo kungathandize munthuyo kuleka njila yake yoipa . ‘ Mulungu sanalenge dziko popanda colinga , koma analiumba kuti anthu akhalemo . ’ — Yesaya 45 : 18 . N’nali kukwanitsa kucita maseŵelawa maulendo ambili popanda kuphonya ciliconse . Sinkhasinkhani mmene ubwenzi wanu ndi Yehova udzalimbila mukadzayamba kukhala angwilo . 11 : 6 ) Yehova anagwilitsila nchito mphamvu ndi nzelu kuti aukitse Yesu ku moyo wosafa wa kumwamba . Mlongo wina anayamikila thandizo limene analandila pambuyo pakuti nyumba yake yaonongeka cifukwa ca cimphepo coopsa camkuntho . Iye anati : “ Ndikuyamikila kwambili kukhala m’gulu la Yehova cifukwa ca thandizo lakuthupi ndi lakuuzimu limene ndalandila . ” ( Danieli 1 : 8 ) Zimenezi zionetsa kuti Danieli anali wofikapo mwakuuzimu . ( Deuteronomo 25 : 16 ) N’cifukwa cake ambili a ife timadana ndi kupanda cilungamo . ( Dan . 1 : 8 ; 6 : 10 ) Komabe , pansi pa ulamulilo wacikunja , zinali zosatheka kwa Myuda woopa Mulungu kutsatila zonse zolembewa m’Cilamulo . Posapita nthawi , munthu wina anabwela ndi kundithandiza kumvetsetsa Baibulo . ” “ Tingakambe motsimikiza kuti palibe zolemba zina zakale zimene uthenga wake unakopedwa mosamala kwambili kupambana Malemba Aciheberi . ” Kodi nimadziŵika monga munthu amene amalimbikitsa mtendele na mgwilizano ? ’ Masiku ano , pali acicepele ambili amene ali ngati Timoteyo . Apa m’pamene atate anakamba mau oopseza amene nafotokoza kuciyambi kwa nkhaniyi . Kukamba zoona , ngati timakonda abale ndi alongo athu sitingacite zimenezi . 8 : 13 ) Kumbukilani kuti timafuna kuyenda ndi Mulungu Wamphamvuzonse , osati mngelo kapena munthu ayi . ( Aroma 2 : 11 ) Kucita zimenezi kungakhale kovuta m’maiko ena . Yesu anafotokoza mfundo imene ingatithandize kuika zinthu zakuthupi ndi zauzimu pamalo ake . ( Mat . 8 : 5 - 10 ) Ndipo m’tauni ya kwawo ku Nazareti , Yesu anafotokoza mmene Yehova anathandizila anthu a mitundu ina , monga mkazi wamasiye wa ku Zarefati , ndi munthu wakhate wa ku Siriya , dzina lake Namani . Coyamba , muzikhala oleza mtima . Kodi anaganiza kuti Mulungu sadzaona zimene anacitazo ? Mwacitsanzo , tingayambe nchito ya malipilo ambili koma imene imatilepheletsa kucita zambili mu utumiki wa Yehova . R . Koma kuti adzalandile colowa cake , afunika kukhalabe wokhulupilika kwa Yehova . ( 2 Tim . 2 : 24 ) Anthu odekha amakhala osamala pocita zinthu ndi ena kuti apewe kuwakhumudwitsa . ( 1 Akor . 6 : 9 , 10 ) Conco , si cikondi kukakamiza m’bale kumwa moŵa ngati iye wakana . Munthu winanso wokhulupilika amene amachulidwa m’Malemba Aciheberi ni Danieli . Davide anatsimikizila Sauli kuti angagonjetse Goliyati . 22 : 15 ) Kholo likanena conco , tingalifunse zimene lingacite ngati mwana wake akanilatu thandizo lililonse . ( Maliko 13 : 14 - 18 ; Luka 21 : 21 - 23 ) Conco nthawiyo isanafike , Akristuwo anafunika kulimbitsa cikondi pakati pao . — Aroma 12 : 9 . Tingaonetse bwanji kuti tikuyembekezelabe mapeto a dongosolo lino la zinthu ? Anthu ena angatione monga tilibe nzelu cifukwa cokhala maso . Koma sitiyenela kuleka kukhala maso . Nditaphunzila zambili , ndinauza Amai kuti ndaleka kucita nao zikondwelelo za Cibuda . Kodi pa Luka 16 : 10 - 13 pali malangizo anji ? Abale na alongo athu ambili aleka makhalidwe oipa amenewa ndipo avala umunthu watsopano . — Ŵelengani Salimo 37 : 8 - 11 . Mwina mufuna citonthozo cifukwa munthu wina amene munali kukonda anamwalila . ( Luka 11 : 52 ) Alembi na Afarisi anali kufunika kuphunzitsa anthu tanthauzo la Mau a Mulungu na kuwathandiza kuyenda pa njila ya ku moyo wosatha . Mmene Mungalangile Ana Anu ? 13 - 15 . ( a ) Kodi mneneli Samueli anapatsidwa nchito yotani ? Conco , aliyense afunika kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ningaseŵenzetse ufulu wanga kuti niwonjezele zocita pocilikiza nchito ya Ufumu ? ’ Malangizo amenewo si ovuta kumvetsetsa . ( Luka 1 : 30 - 32 ; 2 : 52 ) Kodi Mariya anali kudziŵa kuti Yesu ali ndi mphamvu yocita zozizwitsa ? Tsopano , padziko lonse pali Mboni zoposa 7,900,000 , ndipo palinso anthu mamiliyoni amene amagwilizana nao makamaka pamwambo wa Cikumbutso caka ndi caka . Coyamba , Baibo siichula za cikondwelelo ca tsiku la kubadwa la Yesu kapena la mlambili aliyense wokhulupilika wa Mulungu . Pali mtunda wa makilomita pafupifupi 80 kucoka ku mphoto kwa Heburoni kufika ku Sekemu . ( Chivumbulutso 19 : 16 ) N’zoonekelatu kuti monga mfumu yankhondo , iye ali na mphamvu zoculuka , koma saseŵenzetsa mphamvuzo molakwa kapena mosayenela . Kumeneko n’nakumana ndi mlongo wina wakhalidwe labwino , dzina lake Janette ndipo tinakwatilana . Tinabeleka ana anayi , mwamuna mmodzi ndi akazi atatu . N’ciani cimakucititsani cidwi ndi mmene Yesu anali kucilitsila anthu ? N’zoona kuti munthu amapindula ngati acitila ena cifundo . Timamanga ndi kuyang’anila maofesi a nthambi ndi nyumba zosindikiza mabuku padziko lonse lapansi . Imakhalanso nthawi imene munthu amaganizila mozama tanthauzo la kudzipeleka na ubatizo . 5 : 22 , 23 ) Iye anakamba kuti makhalidwe ocititsa cidwi amenewa , onse pamodzi ni “ cipatso ca Mzimu . ” Koma amakamba zimenezi pofuna cabe kudyela anthu masuku pamutu . Anthu ambili panthawiyo anali ndi ciyembekezo cakuti zinthu zidzakhala bwino m’tsogolo . Ndipo ciliconse cimene ndinalanda munthu aliyense pomunamizila mlandu ndibweza kuwilikiza kanayi . ” 14 Ciyembekezo Titamufotokozela kuti Akhristu oona sanyamula zida kuti amenyane ndi anzawo , msilikaliyo anakwiya ndipo anatipeleka kwa mkulu wa asilikali . “ Futukulani mtima wanu . ” — 2 Akor . Kodi n’zoona kuti Mlengi wacilengedwe conse amaona kuti ali na nkhongole kwa anthu amene amacitila anzawo zinthu zacifundo , ndipo adzawabwezela mwa kuwayanja ndi kuwadalitsa ? Nanga n’ciani cingatithandize kukhala ndi cikhulupililo cosagwedela mu Ufumu wa Mulungu ? — Aheb . Koma Mkristu payekha angakumane ndi mayeselo , ndipo ngakhale kuphedwa kumene . Mwacitsanzo , anakapempha thandizo kwa mfumu ya Siriya m’malo modalila Yehova . Komabe , Cigumula sicinacotse kupanda ungwilo , ndipo anthu anali kuvutikabe cifukwa ca cisonkhezelo ca Satana ndi angelo opanduka . Amayi anakhumudwa ndipo ananiletsa kugwilizana ndi a Mboni . Koma ife tinali kuloledwa kucoka ndi kupita kulikonse kumene tafuna . Komabe , panthawiyo , khamu lalikulu linadziŵidwa kuti ndi olambila okhulupilika amene ali ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi la paladaiso . Konzekelani kuti musadzatengemo mbali m’ndale mukadzakumana ndi ciyeso M’paladaiso wathu wauzimu simufunika kumacitika zoipa za mtundu uliwonse . Tifunikanso kulola mzimu woyela kutsogolela maganizo na mtima wathu . Paulo analemba kuti : “ Kuika maganizo pa zinthu za thupi kumabweletsa imfa . ” Tonse aŵili tinayambadi upainiya pa November 1 , 1947 . Yehova analamula kuti Solomo ayang’anile nchito yomanga imeneyi . — 1 Mbiri 22 : 1 , 5 , 9 - 11 . Ganizilani cabe mmene Mose anamvelela pamene Yehova anamuuza kuti : “ Ndikutuma kwa Farao kuti ukatulutse anthu anga ana a Isiraeli ku Iguputo . ” — Eks . Iye anacita ndendende zimene Yehova anamuuza . Mofananamo , kuti cikondi cathu pa Mulungu cipitilize kuyaka , tifunika kumaŵelenga Mau ake nthawi zonse , kusinkha - sinkha zimene taŵelenga , na kulimbikila kupemphela . ( Sal . Conco , Yobu akanafuna , sembe anakwatila mkazi wina . 4 : 3 , 4 ) Mau a Yehova ndi olembedwa m’Baibulo . Mtumwi Paulo anafotokoza kuti magazi ali ndi mphamvu yoyeletsa . Iye analemba kuti : “ Pafupifupi zinthu zonse zimayeletsedwa ndi magazi malinga ndi Cilamulo , ndipo popanda kukhetsa magazi anthu sangakhululukidwe macimo ao . ” ( Aheb . * — Miyambo 8 : 13 . Iwo anadandaula kuti : “ Maso athu sakuonanso kanthu kena , koma mana basi . ” Zili telo cifukwa cakuti Yehova amafuna kuti timudziŵe bwino Mwana wake kotelo kuti titengele makhalidwe ake . Yehova anasiya Aisiraeli ndipo anayamba kuyanja gulu latsopano limene linayamba pa Pentekosite mu 33 C.E . Adamu ndi Hava atacimwa , Yehova anapatsa akerubi ena nchito pano padziko lapansi . N’kupanduka kuti kumene sikunalepheletse colinga ca Yehova ? Conco , tiyeni nthawi zonse tizikhulupilila Yehova ndi kukumbukila kuti “ nkhawa mumtima mwa munthu ndi imene imauwelamitsa , koma mau abwino ndi amene amausangalatsa . ” ( Miy . Tiyeni tione zimene Yesu anakamba . Pamene mtumwiyu anakumana ndi mazunzo ku Yerusalemu , iye anafunsa mkulu wa asilikali wa Aroma kuti : “ Kodi anthu inu , malamulo amakulolani kukwapula munthu amene ndi Mroma , mlandu wake usanazengedwe ? ” Zimene io anacita zinali zosaloleka . Koma Satana sanalekele pamenepo . Ndaligonjetsa dziko ine . ” — Yohane 16 : 33 . Komabe , sanali kudziŵa bwino zimene zimacitika munthu akamwalila . Ndiyeno ine ndinathawa ndi kukwela mumtengo waukulu wa mango . Kutsatila zimene Paulo analemba zokhudza cikondi pocita zinthu ndi anzathu , kungatithandize kupewa mavuto oculuka . Kucita zimenezi kumabweletsa cimwemwe ndipo timadalitsidwa ndi Mulungu . Ngakhale asayansi amene ndi akatswili , sagwilizana pankhani ya cisanduliko . ” Komabe , pamene Yesu anaonekela kwa atumwi ake kotsilizila patapita masiku 40 , io anamvetsetsa tanthauzo la zimene Yesu anakamba m’mbuyomo . Iye anati : “ Mudzakhala mboni zanga mu Yerusalemu , ku Yudeya konse ndi ku Samariya , mpaka kumalekedzelo a dziko lapansi . ” ( Mac . 21 : 25 - 27 ) Kupyolela mwa Yesu Mesiya , ucifumu wa Davide ‘ udzakhazikika mpaka kalekale . ’ Pamene aneba anga anayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova , Ndinadzifunsa kuti : ‘ Kodi dzina lakuti Mboni za Yehova limatanthauza ciani ? Ndinapepesa kwa mkulu wanga Felisa cifukwa comunyoza . Koma iye analimbikila kulimbana naye , ndipo sanafune kum’leka mngeloyo . 4 : 2 - 4 ) Koma anali kugwilitsila nchito mphamvu zake pothandiza anthu ena . Kodi mumaona kuti Ufumu wake ndiwo wokha umene udzathetsa mavuto onse a anthu ? ( b ) N’cifukwa ciani zofalitsa zathu sizifotokoza kwambili zocitika za m’Baibulo ndi zimene zimaimila masiku ano ? Ndi zinthu zabwino ziti zimene mungasinkhesinkhe ? Mtumwi Petulo anayelekezela ubatizo na cingalawa cimene Nowa anamanga . Anati : “ Cofanana ndi cingalawaco cikupulumutsanso inuyo tsopano . Cimeneci ndico ubatizo . ” Yesu anakamba kuti : “ Onse amene ndimawakonda , ndimawadzudzula ndi kuwalanga . ” N’zoonekelatu kuti kutalika kwa Goliyati kunapangitsa kuti asakhale wotetezeka kwenikweni , cifukwa wonyamula zida zake sakanakwanitsa kunyamula cishango pa saizi yakuti ateteze mutu wa Goliyati . N’cifukwa ciani dipo limene Mulungu anapeleka limaonetsa cisomo cake ? Mwacitsanzo , m’bale wina na mkazi wake anali na bizinesi yaikulu imene inali kuyenda bwino . ( Yesaya 11 : 3 , 4 ) Anthu onse amene amakhala nzika za Mfumu Mesiya , ali ndi ciyembekezo cabwino kwambili mu Ufumu wa Mulungu ! — Mateyu 6 : 10 . [ Bokosi papeji 8 9 ] ( 2 Akor . 4 : 2 ; 1 Pet . 1 : 14 ; 5 : 7 ; 12 : 6 - 8 ) Mrabi wina , dzina lake Simeon ben Gamaliel , atakhumudwa na zimenezi , anacepetsa ciŵelengelo ca nsembe zimene Ayuda anafunika kupeleka . Atangocita zimenezi , mtengo wa nkhunda ziŵili unagwelatu . Motelo , sitiyenela kuyembekezela kuti zinthu padzikoli zidzafika poipitsitsa cisautso cacikulu cisanayambe . — Luka 17 : 20 ; 2 Pet . ▪ Kodi Kuukitsidwa kwa Yesu Kumatanthauza Ciani kwa Ife ? Jumpei anakamba kuti : “ Patapita zaka zitatu , ndalama zimene tinasunga zinatsala pang’ono kutha . Kodi Afilipi 2 : 4 ingatithandize bwanji pankhani ya mavalidwe ? M’nyengo yozizila , tinali kucitila m’nyumba misonkhano . Iwo anapitabe ndipo mmodzi anamangidwa , wina anaphedwa . Olo tiyesetse bwanji , patokha sitingakwanitse kum’thaŵa mdani wathu woipitsitsa amene ni imfa . 9 : 22 , 23 . Yehova wasankhanso gulu la otsatila a Yesu kuti akakhale olamulila anzake mu Ufumuwo . — Ŵelengani Luka 11 : 2 ; 22 : 28 - 30 . Iye amanyalanyaza malamulo a Mulungu , ndipo mwa kucita zimenezi , amaonetsa kuti akunyozela Yehova na dzina lake . ( Aheb . 10 : 24 , 25 ) Conco , aliyense amene amadwala cifukwa ca fungo la pelefyumu moti amalephela kufika pa misonkhano angakambilane ndi akulu za nkhaniyo . Angelo si anthu amene anali kukhala padziko lapansi kale - kale . Asilikali a Isiraeli anayamba kufuula ndi kuthamangitsa Afilisiti . Kalatayi imakamba kuti amene anali mboni m’pangano la zamalonda limeneli anali mtumiki wa “ Tattannu , bwanamkubwa wa Kutsidya Lina la Mtsinje . ” 3 : 6 , 17 . M’mau ena tinganene kuti Ufumu umenewu udzalamulila dziko lonse lapansi . Mwacitsanzo , Yehova anaikila Adamu na Hava malile kapena kuti malamulo . Colinga cake cinali cakuti awaphunzitse kulemekeza ulamulilo wake . Sitiyenela kuyembekezela kuti gulu la Mulungu lidzacita kutindandalikila zosangalatsa zoyenela na zosayenela . Sylviana ( kumanzele ) na Sylvie Ann ( kulamanja ) ali na Doratine pa tsiku la ubatizo wake N’ndani amene ni citsanzo cabwino koposa pankhani yokhala wofatsa ndi woleza mtima ? Ndi nkhani zotani zimene tingaphunzile ? Tikacita zimenezo , iye adzatidalitsa . — Ŵelengani Salimo 37 : 5 . Kucita zimenezo kumafuna kudzicepetsa . Palibe munthu amene angakwanitse kutelo pa iye yekha . Iye anati : “ Mwakutelo , onse adzadziŵa kuti ndinu ophunzila anga , ngati mukukondana . ” ( Yoh . Ku sukulu . M’dziko limene Yesu anali kukhala munali anthu ocokela m’madela osiyanasiyana monga a ku Yudeya , Galileya , Samariya ndi kumadela ena . Iye anali kuletsanso Akhristu ena kulandila alendowo . — 3 Yoh . 9 , 10 . Kodi Aisiraeli anakumana ndi mavuto otani cifukwa cogwilizana ndi anthu oipa ? N’ciani cinacititsa atumwi kuona Yesu monga mnzao ? M’kalatayo , munali mau akuti : “ Ucite ciliconse cotheka kuti ubwele kwa ine posacedwa . ” Pa cocitika capadela cimeneco ca mu 33 C.E . , Yesu anagwilitsila nchito mkate wopanda cofufumitsa umene unatsalako pa mwambo wa Pasika . ( Eks . Caka ciliconse , anthu 600 sauzande amene sakoka amafa ndi utsi wa fodya . “ Lolani kuti munthu wa Mulungu woona . . . adzatilangize zoyenela kucita ndi mwana amene adzabadweyo . ” — OWERUZA 13 : 8 . Ndiyeno Yehova anauza Mose kuti : ‘ Igwile kumcila . ’ N’cimodzi - modzi na Nowa . Makopewo anamasulidwa m’zinenelo zambili . ( a ) N’ciani cidzacitika cisautso cacikulu cikatsala pang’ono kuyamba ? Koma simuyenela kuiwala kuti Yehova amayamikila zilizonse zimene mumacita pom’tumikila . Tingaphunzile zambili kwa Yosefe tikaganizila zimene anakamba ndi zimene anapewa kukamba . — Gen . Iye anatsala pang’ono kutaya moyo wake cifukwa coceza mosayenela ndi Ahabu . Iwo anasangalala kwambili pamene anawaitana kuti akaloŵe Sukulu ya Gileadi ya nambala 126 . Ungaseŵenzetse njila yofananayo pokambilana ndi munthu wokaikila za Baibulo . ( 2 Mbiri 20 : 17 ) Koma pakali pano , tili na mwayi waukulu wocilikiza ulamulilo wa Yehova modzipeleka ndi molimba mtima . Tingaphunzile zambili tikamaŵelenga mapemphelo olembedwa m’Baibulo . Mwa kucita zimenezi , timatsatila citsanzo ca Akristu okhulupilika amene akufotokozedwa pa Salimo 99 : 1 - 3 , 5 . Ngati muŵelenga Mau a Mulungu ndi kuwasinkhasinkha , mudzakhala anzelu , ozindikila , acidziŵitso , ndi oganiza bwino . ( Yohane 18 : 33 - 37 ; 19 : 8 - 11 ) Iye anali kuyembekezela nthawi yabwino kuti afotokozele ophunzila ake zinthu zina . 12 : 22 . Conco , kodi n’kutheka kuti Satana anafuna kuti Yesu adziponye pansi kucoka pamwamba pa kacisi weniweni ? Baibulo limanena kuti Mulungu Wamphamvuyonse amathandiza anthu odzicepetsa ‘ panthawi yake . ’ 3 : 17 ) Mau amenewa ayenela kuti anamulimbikitsa ngako Yesu pa utumiki wake wonse wa pa dziko lapansi . Patapita nthawi anakambanso kuti : “ Iyi si nchito ya munthu . ” N’cifukwa Ciani Tiyenela Kusonkhana ? Koma pamene tikuyandikila mapeto a dziko la Satanali , cidzakhala covuta kuti tipewe kutenga mbali m’ndale . Komabe , cingaoneke covuta kutsatila malangizo amenewa . Kodi mumalalikila mwacangu ? Kodi kukhala pa nchito yapamwamba n’kumene kumapangitsa munthu kukhala wacimwemwe ? Kweni - kweni , caputa imeneyo imakamba za odzozedwa . 2 : 13 ) Kukhala odetsedwa kukanacititsa kuti iwo asakhale na mwayi wopezeka pa mwambo wa Pasika , kuphatikizapo pa zikondwelelo na zocitika zina zokhudzana ndi mwambowu . N’cianinso cinathandiza Diane kujaila utumiki wa ku dziko lacilendo ? Mose anati : “ M’maŵa mutikhutilitse ndi kukoma mtima kwanu kosatha , kuti tifuule mokondwela ndi kuti tikhale osangalala masiku onse a moyo wathu . ” Ndiyeno , patapita zaka 4,000 , Yehova modzimana anapeleka nsembe yamtengo wapatali ya Mwana wake wobadwa yekha kuti awombole anthu . ( Yoh . Kodi lemba la Aroma 5 : 12 mungaliike cakumwamba kwa mndandanda wanu ? Kodi cikhulupililo colimba cingakutetezeni bwanji ? Mungapemphele ca mumtima ndiponso m’cinenelo ciliconse . — 2 Mbiri 6 : 32 , 33 ; Nehemiya 2 : 1 - 6 . 39 : 21 - 23 . 27 : 46 ; Luka 23 : 46 ) Mosiyanako , atsogoleli a zipembedzo a m’nthawi yake sanali kulemekeza Mau a Mulungu akaona kuti mauwo akutsutsa miyambo yawo . Zedekiya , mfumu yofooka na yoipa ya Yuda , inalamulila m’nthawi ya mavuto aakulu ku Yerusalemu . Mphatso yamtengo wapatali imeneyi yapangitsa kuti tikhale pa ubwenzi ndi Yehova komanso kuti tizim’konda . Kodi buku la Yobu limatiphunzitsa ciani pa nkhani yolimbikitsa ena ? ( Mlaliki 3 : 1 , 2 ) Komabe , lemba limeneli limakamba cabe za mmene moyo wathu ulili , ndipo limaonetsa kuti palibe angathawe imfa . Ndi malemba ati amene tingagwilitsile nchito pokambitsilana naye nkhaniyi ? Pa nchitoyi tinayenda m’madela okongola a m’mbali mwa mapili a Mulanje m’cigawo ca kum’mwela , mpaka m’madela a m’mbali mwa Nyanja ya Malawi imene ili kum’maŵa kwa dzikoli . Iye amafuna kuti tizikhulupilila kuti Mulungu satikonda ndi kuti sangatikhululukile macimo athu . 3 : 2 ) Zimenezo zikacitika tingayamikile ngati ena atimvetsetsa ndipo aona kuti si mmene tilili . 1 : 14 ) Motelo , Yesu anadzakhala munthu wangwilo monga mmene Adamu analili . Kodi kudziŵa mmene inapulumukila kungakuthandizeni bwanji kukhulupilila kuti Baibulo imene tili nayo masiku ano ni yoona ? Weluzani mopanda tsankho . Ganizilani zimene mukudziŵa tsopano poyelekezela ndi zimene munali kudziŵa zaka 30 kapena 40 zapitazo . Komanso ndisanayambe kulalikila munthu , ndimapempha nzelu kwa Yehova kuti munthuyo ndimufike pa mtima . 15 : 11 - 13 ) Kenako , anawauza kuti : “ Ndakuchani mabwenzi . ” Malangizo ena amene angatipatse angakhale abwino . Kwa zaka mahandiledi ambili , Baibo yapita m’zovuta zosiyana - siyana . Cisumbuci ni ca makilomita 13 muutali , ndipo penapake muufupi , cimafika mamita 500 . Yobu anali ndi cidalilo cakuti adzakhalanso ndi moyo Kodi tsogolo la anthu likanakhala bwanji ngati cikondi silinali khalidwe lalikulu la Mulungu ? Banja lathu silinakhalepo labwino ngati mmene lilili palipano . ” — Viniana . Pemphelani musanayambe kuŵelenga . 31,980 Izi zimalimbikitsa mgwilizano ndi kukambilana momasuka . ( Miy . Zinanitengela nthawi kuti nidzikonze na kukonzekela kukadya cakudya ca m’maŵa . Pa nthawi ina , pamene Yesu anali kuphunzitsa ophunzila ake mfundo yofunika , munthu wina anam’dula mau mwa kunena kuti : “ Mphunzitsi , mundiuzileko m’bale wanga kuti andigaŵileko colowa . ” Mu February , 1984 , ndili pa ulendo wopita ku Lilongwe kuti ndikasiye malipoti opita ku ofesi ya nthambi ya ku Zambia , wapolisi anandiimitsa n’kuyamba kufufuza m’cola canga . Tifuna kuti cikumbumtima cathu cizitikumbutsa miyezo ya m’Baibulo ya cabwino ndi coipa . Ndi mwai wamtengo wapatali kugwila nao nchito yotamanda Atate wathu amene ndi Mpatsi Wamkulu . Ena salabadila kaamba kakuti amakayikila Baibo na Cikhristu cifukwa cokhumudwa na zinthu zoipa zimene anthu ena odzicha Akhristu amacita . ( Ŵelengani 1 Timoteyo 2 : 14 . ) Ngati simufuna kucita kuŵelenga Baibo , mungamvetsele mau a m’Baibo ojambulidwa . Cida cimeneci cinali kupangidwa ndi cikopa cimene cinali kumangidwa ku zingwe ziŵili . MPHAMVU imene tili nayo yokwanitsa kuganizila zinthu zimene sitinazionepo ndi mphatso yocokela kwa Mulungu . N’cifukwa ciani tinganene kuti Kristu anakwela pahachi “ cifukwa ca coonadi ” ? Kucita zimenezo kudzakuthandizani kuyandikila kwambili Yehova . Pamene Cikumbutso cikuyandikila , kodi tingadziyese bwanji ‘ kuti tione ngati tikali olimba m’cikhulupililo ’ ? Muzipepesa mukalakwitsa . Petulo anali kucita usodzi , osati monga cosangulutsa , koma monga njila yopezela zinthu zofunika paumoyo . Acinyamata ena sadziŵa kusiyana pakati pa kudzipeleka ndi ubatizo . ( b ) Kodi anacilimika bwanji ? Nanga anadalitsidwa bwanji ? Akristu odzozedwa , amene asankhidwa ndi Mulungu kukhala ana ake amene adzakhala ndi moyo kumwamba , moyenelela amachula Yehova kuti “ Atate . ” Yesu ayenela kuti anaikidwa pa dengalo . Ananimanga manja kumbuyo n’kuyamba kunimenya ndi nthambo mwankhanza kumapazi . Mavuto amene Yobu anakumana nawo . Masiku ena mungaŵelenge mabuku a Uthenga Wabwino wa Mateyu , Maliko , Luka , ndi Yohane . Iwo amakhulupilila kuti Mulungu adzawononga dziko lapansi leni - leni . Mayi wacigiriki ameneyo anabweleza mau a Yesu na kukamba kuti : “ Inde Ambuye , komatu tiagalu timadya nyenyeswa zakugwa patebulo la ambuye awo . ” N’ciani cinacitika m’caka ca 1914 ? Nanga zimene zakhala zikucitika padzikoli zikutsimikizila ciani ? Ca m’ma 1980 , anayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . Anawapatsanso zonse zimene anali kufunikila , ndipo akanakhala ndi moyo mwamtendele kosatha . ( Gen . Makonzedwe amenewo anacititsa kuti anchito odzifunila azisangalala kutumikila abale ndi alongo ao . 13 KUPATSA KUMAPINDULITSA Iwo amaona ngati kuti kucita zinthu zauzimu ni mtolo osati dalitso . Conco , amaleka kuŵelenga Mau a Mulungu , kupezeka pa misonkhano ya mpingo , na kulalikila . Oyang’anila dela ndi akazi ao amafuna cikondi ndi cilimbikitso cocokela kwa mabwenzi apamtima . 25 : 2 - 13 , 21 , 22 . Palinso mitsinje inayi yocedwa “ Tigrisi , ” “ Firate , ” “ Pisoni , ” na “ Geon ” ku makona anayi a mapuwo . Koma palinso mbali zina za kulambila kwathu zimene zathandiza anthu kudziŵa kuti Mboni za Yehova ndi Akristu oona . Mwini malowo anaona kuti ngakhale kuti banjalo linanamizilidwa , ilo linali kutsatilabe mfundo za m’Baibulo , ndi kupitilizabe kusonyeza ulemu ndi kukhala mwamtendele . Zolakwika monga kusinthanitsa zilembo , mau , kapena ziganizo zimene okopa ena anapanga mosasamala , zikuzindikilidwa mosavuta na kukonzedwa . ( b ) Kodi mphatso imeneyo inawathandiza bwanji ophunzila a Yesu ? 4 FUNSO : Kodi Ufumu wa Mulungu n’ciani ? Tidzakambilana mafunso amenewa m’nkhani ino . ( Mal . 3 : 1 - 3 ) Ndipo mbili imaonetsa kuti zimenezi zinacitika kuyambila mu 1914 mpaka kuciyambi kwa 1919 . Diotirefe anali na mtima wofuna kuchuka komanso wakhalidwe loipa . Izi zinaonetsa kuti anali munthu wosakhulupilika . Kenneth anati : “ Titafika , citseko cinali cokhoma ndipo motoka panalibe . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene Yehova anacitila zinthu ndi Ahabu , Mfumu ya Isiraeli , ndiponso zimene mtumwi Petulo anacita ali ku Antiokeya wa ku Siriya . M’malo mwake , anawauza kuti apite kukagula ao kwa ogulitsa . Koma m’bale wacikulileyo sangachaye bola . Motelo , tiyenela kumakumbukila mau a mphamvu a Mose . 4 : 35 - 38 ) Mofanana ndi mlimi wabwino , Yesu sakanasiya munda umene unali kufunika kukololedwa . 28 Kwa Ine , Kuyandikila Mulungu ndi Cinthu Cabwino 7 : 6 - 27 . Conco , akamafunsa mafunso , timaona kuti zili bwino . N’ciani cinamuthandiza kutsimikiza mtima kuti ili ndi gulu la Yehova ? Mwaona ka ? Yesu anacita kukambanso kaciŵili kuti : “ Musamade nkhawa . ” Pa msonkhano wina wacigawo , mlongo wina anam’citila zinthu zabwino . Olo ana ang’ono - ang’ono angaphunzile kukamba kuti “ conde ” na “ zikomo . ” Susan amanena kuti mau olimbikitsa amene akazi a abale a m’Bungwe Lolamulila amakamba , amamulimbikitsa kuti apitilize kundithandiza mwakhama . ( Chiv . 2 : 10 ; 12 : 17 ) Cina , tifunika kukumbukila nkhani yaikulu imene imalengetsa kuti tizikumana na mavuto amenewa . “ Nkhani yosangalatsa ” imene inakhudza ndi ‘ kugalamutsa ’ mtima wa wamasalimo ndi yokhudza mfumu . N’ciani cingatipangitse kucoka pang’ono - pang’ono kwa Yehova ? 2 : 5 ) Kodi Yesu anali ndi khalidwe lotani ? Baranaba ayenela kuti anali kum’konda Paulo cifukwa anali wacangu ndiponso anali kukamba mosapita m’mbali . Kodi mau a pa Aroma 8 : 5 , 6 akuti kuika “ maganizo pa zinthu ” atanthauza ciani ? Malinga n’zokamba zake , Mdyelekezi anaonetsa kuti anthu angakhale acimwemwe ngako ngati adzilamulila okha . Yesu anagogomeza momveka bwino kuti Yehova sangatikhululukile ngati tilephela kukhululukila abale athu , pamene pali maziko abwino ocitila zimenezo . Mtundu woyamba ni ma IUD okhala na kopa . Mtundu umenewu unayamba kupezeka kwambili ku United States mu 1988 . 4 : 13 - 15 . N’ciani camuthandiza kukhala ndi umoyo wosafuna zambili ? Komabe , kumvela cabe mu mtima kuti tili pa ubwenzi na Yehova kapena kudzionetsela kuti ndise okhulupilika kwa iye , sikutanthauza kuti Yehova akutiyanja . — 1 Akor . ( 1 Yohane 4 : 8 ) Koma kodi zimenezi zitanthauza ciani ? pangano la Ufumu . Takhala ndi mwai wophunzitsa Baibulo anthu ambilimbili . Mwina mungadzifunse kuti : ‘ N’cifukwa ciani kumvela n’kofunikanso ? Muzidzifunsa mafunso . Mofananamo , nthawi zina mungaone kuti zimene mumacita mu ulaliki sizokwanila . Kucokela pamene Yesu anayamba kulalikila , iye anagogomezela kufunika kolengeza uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . Iye anafelanso onse kuti amene ali moyo asakhale moyo wongodzisangalatsa okha , koma akhale moyo wosangalatsa amene anawafela . ” — 2 Akorinto 5 : 14 , 15 . Tsoka likuyenda kucokela mu mtundu wina kupita mu mtundu wina , ndipo mkuntho wamphamvu udzafika kucokela kumalekezelo a dziko lapansi . 18 Kodi Kukhala Munthu Wauzimu Kumatanthauzanji ? M’kupita kwa nthawi , nchito zanu ndi khama lanu zidzadziŵika . ” Alexander Wamkulu atagonjetsa madela ambili , Cigiliki cinakhala cinenelo cofala . POKHALA anthu a Yehova , timakhulupilila kuti mau a Mulungu , amene ndi uthenga wake kwa anthu , “ ndi amoyo ndi amphamvu . ” ( Aheb . Koma panthawi imene sakuiseŵenzetsa , ayenela kucotsamo mpholopolo , kapenanso kuimasula , ndi kuisungila pa malo otetezeka . 137 : 1 - 3 , 6 ) Ayuda sanali kufuna kuimba . 4 : 18 ; Yoh . 16 : 12 . Ndipo nthawi zonse muziyelekezela zimene mwamva ndi “ citsanzo ca mau olondola ” a m’Baibulo . — 2 Timoteyo 1 : 13 . Tinali na nkhawa kwambili pamene tinali kucoka ku America , koma nkhawa yonse inasanduka cisangalalalo pamene abale a ku Nairobi anatilandila pa eyapoti . MABUKU NDI ZOLEMBA ZAKALE zimaonedwa kuti zili ndi maulosi . Filipo wophunzila wa Yesu anati : “ Ambuye , tionetseni Atatewo . ” Coyamba , Baibo imakamba kuti “ Mulungu anatumiza m’dziko Mwana wake wobadwa yekha kuti tipeze moyo kudzela mwa iye . ” Pelekani citsanzo coonetsa kuti Kristu angathe kulamulila mphamvu zacilengedwe . Tingatengele bwanji citsanzo cabwino ca Paulo pankhani yokhala oyamikila ? Mau akuti “ Yehova mmodzi ” atanthauza kuti Yehova ni wapadela , palibe wolingana naye . Cocitika Cimene Simuyenela Kuphonya ( Cikumbutso ) , 3 / 1 Ngati timayesetsa kukhala okhutila , kupempha thandizo kwa Yehova , ndi kucita zomwe tingathe mu utumiki wake , tidzakhala osangalala ndipo tidzalandila madalitso ambili ngakhale tikukhala m’masiku otsiliza . Kusamba m’manja pambuyo pogwila mtembo . Analandila buku limene lili ndi Uthenga Wabwino wa Mateyu wocokela m’Baibulo la Dziko Latsopano . Mlongo wina wa ku South Africa dzina lake Elaine amakumbukila mmene makolo ake anali kumulangizila . Pakati pa anthu amenewa , ambili anaphunzila coonadi , cimene ndi camtengo wapatali kwambili kuposa golide , cakuti anali kufuula kuti “ Eureka ! ” Amagwilitsa nchito nthawi yao , mphamvu zao , cikondi cao , ndi zina zaconco kuti athandize ena . Isaki , mwamuna amene anali ndi zaka pafupifupi 40 , anali akali kulila malilo a mai ake Sara , amene anali atamwalila zaka zitatu zapita . N’ciani cingatithandize kupitiliza kuyenda panjila ya ku cipulumutso ? Mtima wanga umapwetekabe cifukwa ca imfa ya mkazi wanga . Kufulukuta . Mwina munthuyo angaganize kuti madalitso amene akuchulidwa palembali akunena za mmene umoyo udzakhalila kumwamba . Imakambanso kuti : “ Mulungu anamukweza n’kumuika pamalo apamwamba . Akamapempha mzimu wa Mulungu na kuyesetsa kukulitsa makhalidwe amene mzimuwo umabala , amakhala dalitso kwa abale awo . ” — Sal . Conco , munthu akanatha kuthaŵilako mwamsanga ndi mosavuta . — w17.11 , peji 14 . Cifukwa cakuti mtsikanayo anafunika kukatumikila pa cihema , sakanakhala ndi ana . Colinga cake ceni - ceni cingakhale kupita paulendo na banja lake kupikiniki . Kuyambila pamene kapolo wokhulupilika anaikidwa mu 1919 , mamiliyoni a “ anchito apakhomo ” ocokela m’zinenelo zonse abwela m’gulu la Mulungu , ndipo akudyetsedwa mwa kuuzimu . Tinali kutenga ana athu popita mu ulaliki na ku misonkhano ya mpingo . “ Idzafika nthawi pamene onse ali m’manda acikumbutso adzamva mau ake ndipo adzatuluka . ” — Yohane 5 : 28 , 29 . [ Cithunzi papeji 6 ] “ Lazaro , tuluka ! ” Abale anali ofunitsitsa kunithandiza kuti niphunzile , ndipo nimawayamikila cifukwa ca kuleza mtima kwawo na kuniwongolela moona mtima . 29 Ndili pa Mtendele ndi Mulungu Komanso ndi Amai 5 : 7 ) Ndithudi , tonse timafunika kukhala woleza mtima . Ofalitsa ambili aona kuti kuseŵenzetsa Mau a Mulungu mu ulaliki kumawakhudza ngako anthu amene timawalalikila . Mwacitsanzo , ganizilani zimene mai amene wabeleka mwana anafunika kupeleka . N’zoona kuti kupeza mphatso yaconco kumakhala kovuta , komabe kuganizila mfundo zina kungakhale kothandiza . N’cifukwa ciani timakonda Yehova Mlengi wathu ? 147 : 10 ) M’malomwake , tifunika kucondelela Yehova kupitila m’pemphelo kuti atithandize . Pamene anaphunzila kupemphela , ndinali kuwalimbikitsa kuti azipemphela mokweza n’colinga cakuti ndimve mmene amafotokezela maganizo ao kwa Yehova . Nimam’dalila kwambili ngakhale tikumane na mavuto aakulu . Iwo anangopitiliza kugaŵila magazini anthu amene anali kutamba zimene zinali kucitika . Ni mphoto yanji imene anthu amene amayamikila cisomo ca Mulungu adzalandila ? ( Mac . 16 : 4 , 5 ) Kalata yokhudza cigamulo cawo imene analemba ionetsanso kuti bungwe lolamulila linali ndi cipatso ca mzimu wa Mulungu monga cikondi na cikhulupililo . — Mac . 15 : 11 , 25 - 29 ; Agal . Anati : “ Musamagwile nchito kuti mungopeza cakudya cimene cimawonongeka , koma kuti mupeze cakudya cokhalitsa , copeleka moyo wosatha . ” — Yoh . 6 : 25 - 27 . TSAMBA 18 • NYIMBO : 36 , 51 Mwacitsanzo , iye anathandiza pa phwando la cikwati ku Kana mwa kusandutsa madzi kukhala vinyo wabwino . 13 , 14 . ( a ) N’ciani cingaonetse kuti mwana wanu wacinyamata afunika kulimbitsa cikhulupililo cake ? ( Mac . 5 : 37 ) Ndipo Azeloti ena anali kucita zaciwawa pofuna kukhala na ufulu wodzilamulila . Nthawi zina umoyo umakhala wosiyana kwambili ndi mmene tinali kuganizila pamene tinali acicepele . Baibo imati : “ Gonjelani Mulungu , koma tsutsani Mdyerekezi ndipo adzakuthawani . ” Iye anafotokoza zimene zinam’thandiza kukhala wacimwemwe pamene anati : “ Ndimalalikila kudela kumene anthu ambili amamvetsela uthenga wabwino . 22 Ubwino Wotsatila Malangizo a Yehova Coyamba , ndinaganiza kuti pambuyo pa miyezi itatu ndidzakhalabe wofunitsitsa kutumikila Yehova . Koma sitingathe kumuona ndi maso athu monga mmene Petulo anacitila . Yesu , amene ndi mutu wa mpingo anati : “ Kulikonse kumene aŵili kapena atatu asonkhana m’dzina langa , ine ndidzakhala pakati pao . ” Conco , iye amaseŵenzetsa dziko lakeli kugwetsa anthu mphwayi kuti asamaŵelenge ndi kuphunzila Baibo . Nanga ndani makamaka amene sangakhululukidwe ndi Mulungu ? Ndinauzidwa kuti a boma andilipilila maphunzilo a ku yunivesite . Ngati iwo atipatsa uphungu pa mbali zimene aona kuti siticita bwino , kodi timamvela na kuseŵenzetsa uphunguwo ? Ngati ticita zimenezi , tidzaonetsa kuti timakonda Yehova , ndi kuti timafuna kuti mau ake ‘ aziunikila mapazi athu . ’ ( Sal . 21 “ Udalitsike Cifukwa ca Kulingalila Bwino Kwako ” ( Yakobo 4 : 8 ) Conco watiuza dzina lake . ( b ) Kodi Paulo anali kuuza anthu kuti ni kwa ndani kumene akanapeza ufulu weni - weni ? Gulu la nkhondo la Sisera ndi magaleta ake ambili anacititsa mantha dziko lonse . Iwo anayenda kudutsa cigwa uku akukuwa kwambili . Nkhondo ya Aramagedo ikadzatha , padzikoli padzacitika zozizwitsa zambili . • N’cifukwa ciani zinthu zoipa zimacitikila anthu abwino ? Tsopano , Adamu ndi Hava anafunika kusankha coyenela kucita . Imeneyi ndi njila imodzi imene tingaonetsele kuti sitikupeputsa zimene timakhulupilila . Kodi Yehova Mulungu amaona kuti mbali zocepa kwambili n’zofunika ? Pamene n’nali ndi zaka pafupi - fupi 9 , amayi anayamba kupita ku holo kumene Ophunzila Baibulo [ dzina lakale la Mboni za Yehova ] anali kucitila misonkhano yawo . Kuganizila kwambili mfundo zamtengo wapatali zopezeka m’buku la Levitiko , kwatithandiza kumvetsetsa cifukwa cake tiyenela kukhala oyela . Kodi mumafuna kucita cifunilo ca Yehova kuposa cinthu cina ciliconse ? Warren Buffett , mmodzi mwa anthu olemela padziko lonse lapansi , amalosela zamalonda molondola cakuti anthu ena amamucha kuti ndi mneneli . Tsiku lina , mu May 1955 titafika panyumba kucokela mu utumiki , ine na M’bale Leach tinapeza makalata m’cipinda cathu . Nanga n’cifukwa ciani iye walola kuti nkhaniyi ipitilizebe mwa kupatsa Satana nthawi yotsimikizila kuti zokamba zake n’zoona ? Anauza atate ake kuti : “ Ndicitileni mogwilizana ndi zimene zatuluka pakamwa panu . ” Ndiyeno , tsiku lotsatila pamene ndinali mu utumiki , alongo aŵili anandipempha kuti ndiyambe nchito yophunzitsa ana ao . Yehova Mulungu anawapatsa mfundo zabwino zimene zinali kuwathandiza kupanga zigamulo zoyenela . 3 : 1 ) Komabe , abale ena amaopa kukalamila maudindo . 24 : 45 ) Koma tidziŵa bwanji kuti Yehova ndiye akutitsogolela kupitila mwa Mwana wake wosaoneka ? N’cifukwa ciani zili na malamulo amene amazitsogolela ? Kunama ni kukamba cinthu cimene si coona . Kristu mwini wake anati , ngati wina sanabadwenso ndi madzi ndi Mzimu Woyela , munthuyo sadzaloŵa mu Ufumu wa Mulungu . ” Ngati muli ndi cikhulupililo colimba , mudzakhala ndi ‘ makhalidwe oyela ndi kucita nchito zosonyeza kuti ndinu odzipeleka kwa Mulungu . ’ ​ — Ŵelengani 2 Petulo 3 :⁠ 11 . N’ciani cinacitika patsiku la ubatizo wanu ? 2 : 9 , 10 ) Kukamba naye mwacikondi , kungamuthandize kuwongolela . Mulungu wokhulupilika , amene sacita cosalungama . Iye ndi wolungama ndi wowongoka . ’ — Deut . Abulahamu sanangosiila mkazi wake kugwila yekha nchitoyo . Iye anathamanga kukapha ng’ombe yaing’ono , ndipo anakonza zakudya na zakumwa zambili . Pewani kugula zinthu zosafunika kweni - kweni . Amaphunzila kuti ufulu uli na malile , na kuti khalidwe lathu na zosankha zathu zimakhala na zotulukapo , kaya zoipa kapena zabwino . Koma popeza kuti Aiguputo akale anali kutumiza nsomba zouma ku Siriya zikuonetsa kuti njila zimene anali kugwilitsila nchito zinali zabwino . [ Cithunzi papeji 13 ] Poyamba , sitinali kumvetsa ngakhale pang’ono zimene munali kukamba . ” Mlimi wa mitengo ya maolivi amafunitsitsa kuti mizu ya mtengo umene anadula iphukenso . Nayenso Yehova Mulungu amalakalaka kuukitsa atumiki ake ndi anthu ena ambili amene anafa . ( Mat . 22 : 31 , 32 ; Yoh . 5 : 28 , 29 ; Mac . Kwa caka cimodzi , n’nagwilizana ndi abale atatu kulalikila anthu odula mitengo omwe anali kukhala m’gawo losalalikidwa , kumpoto kwa Ontario . ( Yes . 62 : 6 ) Alondawo anafunika kukhala maso nthawi zonse . Onani Nsanja ya Mlonda ya Cizungu ya May 1 , 1956 , masa . 269 - 272 , na ya March 15 , 1971 , masa . 186 - 190 , kuti mudziŵe za nchito ya umishonale ya banja la Steele . Iwo anali kutiuza za ciyembekezo codzakhala ndi moyo m’paradaiso pa dziko lapansi . ( Onani danga lakuti “ Tiyeni Tipitilize Kufuna - funa Anthu Oyenelela . ” ) ( b ) Tidzakambilana mbali iti yokhudza dipo m’nkhani yotsatila ? 2 : 2 , 3 . “ Mwati mudziŵa zaka zanga , ” ? 97 : 1 . 1 : 3 , 4 ; 1 Ates . 4 : 13 ) Tikadwala kwambili kapena tikavulala , timamva ululu , koma timapewa kulandila cithandizo ca mankhwala cimene sicigwilizana ndi mfundo za m’Baibulo . ( Mac . Munthu wokonda cuma amadziŵika mwa kuona zimene amalakalaka , zimene amafuna kucita , ndi zimene amaika patsogolo mu umoyo wake . Koma nthawi imeneyo sindinadziŵe kuti posacedwa ndidzakhala mbali ya ubale weniweni , umene ndi ubale wa kuuzimu . INDE , nthawi zina . N’zoona kuti panali zovuta zina . 2 : 9 , 10 ) Conco , colinga ca mtunduwo cinali kukhala mboni za Yehova zolimba mtima , mwa kulengeza poyela kuti iye ndi Mfumu ya Cilengedwe Conse . 7 : 15 ) Apa satanthauza kuti Mkhiristuyo tsopano ni womasuka kukwatila , yayi . Komanso , safunikila kucitoumiliza wosakhulupililayo kuti asacoke , yayinso . UTUMIKI wathu ndi wofunika kwambili ndipo ndi wamtengo wapatali . Izi zidzatithandiza kupanga zosankha zom’kondweletsa ndi kutsatila citsogozo cake . — Ezekieli 11 : 19 . Komabe , Yesu sanali kukonda kwambili zosangalatsa . Inali nthawi yokondweletsa ngako . 4 : 6 , 7 ) Conco , mukakhala ndi nkhawa ganizilani thandizo limene Yehova amapeleka kuti atithandize kulimbitsa ubwenzi wathu ndi iye . Limodzi naye panali enanso 144,000 olembedwa dzina lake ndi dzina la Atate wake pamphumi pao . . . . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Cabwino cimene ungacite cisakhale cokukakamiza , koma ucite mwa kufuna kwa mtima wako . ” — Filimoni 14 . ( Aheb . 6 : 17 - 20 ) Monga mmene nangula amacilikizila ngalawa ku mphepo yamkuntho , ciyembekezo cathu codzalandila mphoto cingatithandize kukhala osagwedezeka m’maganizo ndi mwauzimu . “ Wothilila ena mosaumila nayenso adzathililidwa mosaumila . ” — Miy . ( Yak . 2 : 19 , 20 ) Komabe , pokamba za munthu wina wakale wa cikhulupililo , Yakobo anafunsa kuti : “ Kodi Abulahamu atate wathu sanayesedwe wolungama cifukwa ca nchito zake , atapeleka Isaki mwana wake nsembe paguwa ? 42 : 11 ; Aheb . Komabe , ena zimawavuta kulimvetsetsa . ( Miyambo 14 : 30 ; 27 : 4 ) Kodi munacitapo nsanje mutaona kuti winawake waonetsedwa cikondi kapena kupatsidwa ulemu umene inu munali kuuyembekezela ? Ndipo ndinadziona kukhala wapamwamba kuposa anzanga , koma ngakhale zinali conco ndinalibe cimwemwe . ” ( Ŵelengani 1 Akorinto 12 : 12 , 18 , 21 - 23 . ) N’cifukwa cake Baibulo limatilimbikitsa kuti tiyenela kuyesetsa kukhala ndi khalidwe limeneli . Mufunika kukhala oleza mtima na kudzipatsa nthawi yokwanila yakuti mujaile . Kaamba ka zocitikazo , woyang’anila ndendeyo ndi onse a m’banja lake anabatizika . Kondwelani , dumphani ndi cimwemwe , cifukwa mphoto yanu ndi yaikulu kumwamba , pakuti umu ndi mmenenso anazunzila aneneli amene analipo inu musanakhaleko . ” — Mat . Panthawiyi ndinali kukhala ndi cisumbali canga cimene cinali kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . Kodi cikhulupililo canu ndi colimba cakuti cimakucititsani ngati kuti ‘ mukuona Mulungu ’ ? ( 2 Maf . 18 : 22 - 25 ; 19 : 6 ) Ndiyeno , iye anatumiza mngelo amene anapha asilikali Aasuri 185,000 pa usiku umodzi cabe . — 2 Maf . Ndikatelo ndimamva bwino , ndipo ndimapitilizabe kukonda Yehova . ” Akulu amene amaganizila zamtsogolo mwa kuphunzitsa abale ena amaonetsa kuti ndi oyang’anila anzelu ndipo mpingo wonse umapindula . NYIMBO : 60 , 64 16 , 17 . ( a ) N’ciani cimene tiphunzilapo pa malangizo a pa Mlaliki 11 : 6 ? ( Ŵelengani Luka 4 : 43 . ) Kungocokela pa tsiku loyamba , n’nalembetsa kampani yanga ndipo n’malipila misonkho yonse . ” — 2 Akorinto 8 : 21 . ( a ) N’cifukwa ciani ndi ngozi kugwilitsila nchito dzikoli mokwanila ? Sukuluyi manje inaloŵedwa m’malo na Sukulu ya Alengezi a Ufumu . Komanso , musamangololela zilizonse zimene anawo apempha . Mu 1943 , n’naloŵa Sukulu ya Ulaliki , imene inangoyamba kumene . Gary Yobu anali kudziŵa kuti Mulungu amafuna kuukitsa akufa . N’ciani cingakuthandizeni kuti muzimvela ena cifundo ? Sitingasankhe ziphunzitso zimene tingatsatile . — Yak . ( Zek . 6 : 14 ) Mofananamo , Yehova sadzaiŵala ngakhale pang’ono zonse zimene timacita pom’tumikila , ndi cikondi cimene timamuonetsa ! — Aheb . 6 : 10 . Matanthwe aconco amakhala na tumphako mkati , ndipo amasunga madzi cakuti anthu angathe kuwabowola kuti apeze madzi . Asilamu a ku India anathaŵila ku Pakistan , ndipo Ahindu na Asikhi a ku Pakistan anakakhala ku India . Limati Esau ‘ sanayamikile zinthu zopatulika , ’ ndipo “ anapeleka [ kwa Yakobo ] udindo wake monga woyamba kubadwa pousinthanitsa ndi cakudya codya kamodzi kokha . ” Koma cifukwa ca nthawi yofupikayo , anafunika kuika patsogolo zinthu zauzimu . — Mat . Mukayanjananso na munthuyo , mudzakhala na mtendele wa m’maganizo . — Mateyu 5 : 23 , 24 Kukamba zoona , umoyo wokhala wokhumudwa na kusunga cakukhosi , si umoyo wacimwemwe ndipo umaononga thanzi . Pali pano , Oliver na mkazi wake , Anna , akutumikilabe mwakhama m’gawo la Chichainizi . Cokani pamaso panga , anthu osamvela malamulo inu . ’ ” — Mateyu 7 : 21 - 23 . ROBERT anabatizika ali wacicepele , koma anali kucitenga mopepuka coonadi . Gidiyoni anafuna kudziwa kuti adzakwanitsa bwanji ‘ kupulumutsa Isiraeli m’manja mwa Amidiyani . ’ Tikamatengako mbali pa nchito yopanga ophunzila , timaonetsa kuti ndife omvela . — Mat . Pamene Yesu anakamba kuti tizipempha cakudya cathu calelo , anali kutanthauza kuti tiyenela kupempha zofunika za pa umoyo . Sankhani maina angapo , ndipo pemphani Yehova kuti athandize abale ndi alongo amenewa kukhalabe olimba ndi okhulupilika kwa iye . — Aefeso 6 : 19 , 20 . Kodi tingawalimbilitse bwanji ena ? Ukatelo , udzakhala ndi moyo wopambana , ndipo udzacita zinthu mwanzelu . ’ — Yos . Baibo imaonetsa kuti anthu okonda Mulungu amakhala ‘ acimwemwe , amtendele , oleza mtima , okoma mtima , abwino , a cikhulupililo , ofatsa ndi odziletsa . ’ ( Agal . Zakudya , zakumwa , ndi zovala n’zofunika kwambili mu umoyo . A Zulu : Mwacidule ulosiwu uli ndi kukwanilitsidwa kwa mbali ziŵili . ( Salimo 91 : 11 ) Anthu ena amakhulupilila kwambili kuti Mulungu amawateteza na kuwatsogolela kupitila mwa angelo . Iye anali ndi mphamvu zowapha nthawi imeneyo . Komanso , mizela yobadwila ya Yesu imene Mateyu na Luka analemba imasiyana . Debora ananenelatu kuti mkazi osati Baraki , ndiye adzalandila ulemelelo , cifukwa cogonjetsa Akanani . Komabe , “ Nowa anayanjidwa ndi Yehova ” cifukwa cakuti “ anali munthu wolungama . ” “ MATENDA amandilepheletsa kucita zambili mu utumiki , ” anatelo modandaula Ernst wa zaka za m’ma 70 . Iye anali kudziona ngati wosafunika , moti nthawi zina anali kuona kuti Mulungu sangamukonde . Motowo unafalikila mwamsanga m’madela ambili ndipo unaononga mitengo pafupifupi 2 biliyoni . Kodi Yehova anam’thandiza bwanji Davide kupilila mavuto amene anakumana nawo ? Citsanzo cimodzi ca m’Baibulo ndi ca mneneli Eliya . Paulo anali kuyamikilanso kwambili Akristu anzake , ndipo anali kukonda kuyamikila Yehova cifukwa ca makhalidwe abwino ndi cikhulupililo ca Akristu anzakewo . ( Afil . Yesani kumufunsa funso lokhudza mtima lakuti : ‘ Muganiza kuti Yehova anamva bwanji pamene munabatizidwa ? ’ ( Miy . Ngakhale kuti Baibulo limaonetsa kuti munthu wina anali kudzaimila munthu winawake mtsogolo , sitiyenela kuganiza kuti nkhani iliyonse kapena cocitika ciliconse cimaimila cinthu cacikulu codzacitika mtsogolo . Tiyeni tikambilane mafunso atatu amene tachula pamwambapa kuti tione mmene ziyeneletso zimenezo zingatithandizile . 6 : 22 , 23 . Conco , itafika nthawi yakuti mpingo wawo wa Cixhosa ulandile abale a mpingo wa Cizungu , Noma anakonza cakudya na kuitanako ena mwa alendowo . Carolina , amene anasamukila m’dziko lina pamodzi na makolo ake , anati : “ Nimakondwela ngako kutumikila mumpingo wa citundu ca m’dziko limene tinacokela . M’kupita kwa nthawi , anthu anayamba kuseŵenzetsa liu limeneli pofuna kukamba za munthu amene amacita zinthu mwacinyengo kuti apeze zimene afuna . Khalani odzicepetsa ndiponso ololela . — Afil . Kuganizila mozama za ubwino wa Yehova nthawi zonse , kungatithandize kukhulupilila kwambili kuti ulamulilo wake ndiwo wabwino koposa . Iye anati : “ Mmene nyumbayi ikuonekela zionetsa kuti cipembedzo canu n’coona . ” Koma mkati mwa nthawi “ yokolola ” kapena kuti nthawi ya mapeto , nchito yolalikila inali kudzayambanso kugwilidwa mwakhama . ( Mat . M’maiko olemela , akulu akukumana ndi vuto lina la mmene angathandizile abale obatizidwa a zaka za m’ma 20 kapena za m’ma 30 kutengako mbali m’nchito za mumpingo . ( Aroma 6 : 13 ) Paulo anali wotsimikiza kuti anthuwo akhoza kukhalabe oyela mwauzimu , ndi kupitiliza kupindula na cisomo ca Mulungu . Kodi ena mwa madalitso amenewa ni ati ? Cinsinsi Namba 10 Kudalilika Ngakhale n’telo , timaona kuti ziphunzitso za m’Baibulo zimapulumutsa miyoyo ya anthu . Yesu anaphunzitsa otsatila ake mfundo yofunika imene imatithandiza kukhala ogwilizana . ( Luka 23 : 53 ; Yoh . 19 : 41 ) Conco , Yosefe anaonetsa kuwoloŵa manja kwakukulu mwa kuika Yesu m’manda ake am’tsogolo . Mwacitsanzo , ganizilani zimene zili pa Aefeso caputala 5 . Misonkhano imatilimbikitsa . Panthawi ya nkhondo yaciŵili ndi pambuyo pake , ndi kaimidwe kotani kamene Mboni za Yehova zinatenga ? ( b ) Ndi tumapepala tuti tumene mwaona kuti ndi tothandiza ? Ayenelanso kuti amadzimana zinthu zambili zotaitsa nthawi ndi zosokoneza maganizo ake n’colinga coti asadzipanikize pocita pulakatisi . Vinyo umene Yesu anagwilitsila nchito pa Nisani 14 mu 33 C.E . , unaimila magazi ake , mofanana ndi vinyo umene timagwilitsila nchito pa Cikumbutso masiku ano . Mofananamo , cikhulupililo cathu ‘ cimaonjezeka ’ tikamaphunzila za Mulungu komanso tikamacita “ zinthu zomukondweletsa , ” ndipo timalandila thandizo lake . ( b ) Nanga kungatithandize bwanji pa nkhani ya mavalidwe ndi kudzikonza , ndiponso pa khalidwe lathu ? N’ciani cingapangitse abululu athu osakhulupilila kutitsutsa ? Nanga tingaonetse bwanji kuti timawaganizila ? Kodi mfundo za m’Baibo n’ciani ? Nanga Yesu anaziseŵenzetsa bwanji pophunzitsa ? Mbili ya mmene Mulungu anali kucitila zinthu ndi anthu ake ionetsa kuti iye amaonetsa cikondi cake cokhulupilika kwa “ anthu amene amam’konda ndi kusunga malamulo ake . ” ( Deut . ‘ Kodi nimakalipa msanga ? ’ Covalaco cinali kupangitsa kuti iye asamakhale womasuka kweni - kweni poyenda , ndipo nthawi na nthawi anali kufunikila kumaona ngati tunsimbito tukali togwila bwino . Popeza sitikhoza kudziŵa za mumtima wa munthu , tiyenela kupewa kuganizila molakwa zolinga za anthu ena . — Ŵelengani Yakobo 4 : 12 . Ngati mwamvela mfundo inayake imene muona kuti ingafooketse cikhulupililo canu , muzifufuza m’Mau a Mulungu kuti mudziŵe zimene amakamba pa nkhaniyo . Kodi anthu ena akamba ciani ponena za Mboni za Yehova ? Pothawa , zigaŵengazo zinanitenga n’kuloŵela kumapili a kufupi na dziko la Albania . Nthawi zambili timakumana ndi zopanda cilungamo zimene zimavuta kuzipilila . Nditafika zaka 14 , ndinali nditaphunzila kale njila zambili zonamizila anthu . Kuti mudziŵe zambili zokhudza colinga ca Mulungu codzaukitsa akufa , onani Nkhani 7 m’buku yakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse , yofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . Dipo — ‘ Mphatso Yangwilo ’ Yocokela kwa Atate , Feb . Koma kuti aikidwe kukhala mfumu ya mtundu wake cabe , anafunika kuyembekezela kwa za 15 . ( 2 Sam . Susan anali pakhonde kunyumba ya makolo ake ku Cranston Rhode Island . Mlongo winanso wa ku Central Europe anati : “ N’nali watsankho , n’nali kuzonda munthu aliyense amene sanali wa m’dziko lathu kapena amene sanali wacipembedzo canga . ” Panthawi ya Ulamulilo wake wa Zaka Cikwi , Kristu adzakhalanso tate wa anthu ena . Kwa zaka 17 , ndinali kupemphela kuti ndipeze mayankho a mafunso anga . 5,600 Pokambitsilana , mungagwilitsile nchito mfundo zili pa khadi la DPA la Mboni za Yehova . Baibo imakamba kuti mtendelewo ‘ udzateteza mitima yathu ndi maganizo athu mwa Khristu Yesu . ’ ( Afil . Cifukwa cosamvetsetsa cinenelo , anawo sapindula ndi misonkhano . Kodi nthawi zina mukamakumana ndi mavuto mumadzimva kuti muli nokha ? Dzina la Pilato limapezeka nthawi zambili m’mabuku a wolemba mbili yakale waciyuda wochedwa Josephus . Iye analemba zocitika zitatu pofotokoza za mavuto amene Pilato anakumana nao polamulila Yudeya . PANTHAWI ya ulamulilo wa Mfumu Yerobowamu , Yehova anatuma mneneli wa ku Yuda kukapeleka uthenga waciweluzo kwa mfumu yopandukayo ya Isiraeli . Tikukhala m’nthawi “ yapadela komanso yovuta , ” pamene anthu ambili ali ndi nkhawa zoculuka . Komanso pa Yona 1 : 4 pamati : “ Yehova anabweletsa cimphepo camphamvu panyanjapo , ndipo panacita mkuntho wamphamvu . Iye anati : “ Zinandivuta kwambili kuti ndiuze mkazi wanga ndi akulu zimene ndinali kucita . Ndithudi , ngakhale munthu mmodzi wocimwa akalapa na kubwelela kwa Yehova , “ kumakhala cisangalalo coculuka kwa angelo a Mulungu . ” — Luka 15 : 10 . Tiyelekezele motele : Pambuyo pakuti cakolwa wamwa moŵa kwambili , angakhale woseka - seka . Peter anayankha kuti : “ Mbali ina inalembedwa m’Ciaramu . ” PACIKUTO : Ofalitsa a ku Italy amene amasonkhana ndi mpingo wa cinenelo ca Cichaina , akulalikila alendo odzaona malo mumzinda wa Rome . Ngati mumalakalaka kutumikila monga mkulu , koma zimenezo sizicitika ngakhale kuti papita zaka zambili , pitilizani kudalila Yehova . ( c ) Kodi Yehova amatidalitsa motani ? Koma anakhalabe pa ubwenzi wabwino ndi Atate wake ndipo anapitilizabe kuwatumikila mokhulupilika . Tidzakambilananso zimene tingaphunzile kwa amuna ndi akazi okhulupilika akale pankhani yombekezela Mulungu moleza mtima . ( Ezara 1 : 1 - 3 ) Mulungu ndi yekhayo amene akanalosela ulosiwu . Mofanana ndi zolengedwa zauzimu zolungama kumwamba , nyenyezi zinalengedwa mocititsa cidwi kwambili . Kodi gulu la kumwamba la Yehova alifotokoza bwanji m’buku la Ezekieli ? Kapena kodi cidzayamba kutha pang’onopang’ono ? ’ Zimenezo zimandithandiza kukhala ndi ciyembekezo . ” Kodi iye watilonjeza ciani ? N’cifukwa ciani adani a Isiraeli analephela kuona dzanja la Mulungu ? ( Mac . 20 : 21 ) Citsanzo ca Paulo cingatithandize bwanji pamene tikonzekela kukalalikila anthu onse a m’gawo lathu ? — 1 Tim . Nkhaniyi ifotokoza bwino cifukwa cake sititengamo mbali m’mikangano ya dzikoli ndiponso mmene tingaphunzitsile maganizo athu ndi cikumbumtima cathu kuti tisamatengemo mbali m’mikangano imeneyi . Ndiye cifukwa cake ine ndi mkazi wanga tinayamba kuzungulila dziko lapansi . Kodi muganiza kuti Yosefe anamva bwanji ? Nanga ife tiphunzilapo ciani pa cikhulupililo cake masiku ano ? Mfumu Sauli anasankhidwa ndi Yehova , koma anacitila mwana wake zinthu zoipa . Komanso kwa nthawi yocepa , ndinaseŵenzako kwa amene anagula wailesi ya WBBR , imene iwo anayamba kuicha WPOW . Iye anavulazidwa pa nkhondo ndipo anafela m’galeta lake . Satana ananenanso kuti Mulungu amamana anthu ufulu wosankha okha cabwino ndi coipa . Ponena za Isiraeli wa kuuzimu , amene anali kudzakhala m’pangano latsopano , Yehova analosela kuti : “ Ine ndidzakhala Mulungu wao ndipo io adzakhala anthu anga . ” — Yer . N’zoona kuti Basa analeka kulimbana ndi Asa . Tiyeni tikambilane nkhani yogaŵila maudindo pa mbali ziŵili . Mvula inali itayamba kugwa ndipo alimi anali kulima minda yao . Tiyenela kuthandiza anthu amene timaphunzila nawo Baibulo kudziŵa mfundo imeneyi . Mungatulile bwanji Yehova nkhawa zanu kupitila m’pemphelo ? Anati : “ Ndikudziŵa kuti adzauka pa kuuka kwa akufa m’tsiku lomaliza . ” ( Yoh . Monga mwa nthawi zonse , “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” ndiye ali ndi udindo waukulu wopeleka cakudya kwa anchito apakhomo . Patapita nthawi , Yehova anaonetsa mphamvu zake ndi ulamulilo wake pa Farao wouma khosi . Njila imodzi imene Yehova amatipatsila cakudya ca kuuzimu ndi kudzela m’misonkhano ya mpingo imene timakhala nayo mlungu ndi mlungu ku Nyumba ya Ufumu . N’cifukwa ciani zinali zosavuta kuti ophunzila azipanga maulendo mu Ufumu wa Aroma ? Conco cinjokaco cinaponyedwa pansi , njoka yakale ija , iye wochedwa Mdyerekezi ndi Satana , amene akusoceletsa dziko lonse lapansi kumene kuli anthu . Iye anaponyedwa kudziko lapansi , ndipo angelo akenso anaponyedwa naye limodzi . ” — Chivumbulutso 12 : 7 - 9 . Tiziwapemphelela ndi kucita zinthu mogwilizana ndi mapemphelo athu . Ndipo anthu ena makolo ao samawadziŵa n’komwe . Mwacitsanzo , zingakhale kuti iye analeka kupemphela , kulalikila , ndi kusonkhana . Pamene anali kuphunzila Baibulo , anali kuuzako a m’banja lake zimene anali kuphunzila . Koma anthu ambili a Mulungu alibe maganizo otelo . 6 : 15 - 17 ) Yankho timalipeza m’caputala 7 ca buku la Chivumbulutso . Kwa ine , malo odyela analibe kanthu . Timapeza anthu ambili acidwi . 13 : 36 ; Maliko 7 : 17 ) Caciŵili , io anali okonzeka kuphunzila zambili kuonjezela pa zimene anali kudziŵa kale . Cikondi cake pa ife cimatipatsa cidalilo cakuti colinga cake cokhudza anthu cidzakwanilitsidwa m’njila yabwino kwambili . Mwankhanza Atsogoleli acipembedzo a Afalisi ndi a Asaduki anatsutsa Yesu , ngakhale kufuna kumupha . Kumbukilani kuti kuleza mtima ni khalidwe limene mzimu woyela umatulutsa . ( Aef . Mulungu amatikhululukila macimo . Umu ndi mmene iye anakonzela podzayankha kuti inde . Ndipo tiyenela kupempha mzimu woyela cifukwa Yesu anatitsimikizila kuti , “ Atate wakumwamba adzapeleka moolowa manja mzimu woyela kwa amene akum’pempha . ” — Luka 11 : 13 . Ngati inu a bwanamkubwa simuona kuti ni udindo wanu kumuuza kuti abweze covala ca mtumiki wanu , mucite zimenezi cifukwa conimvela cifundo . Ndi njila imodzi iti imene Yehova amasonyezela kuti ndi Mpatsi wa “ mphatso iliyonse yabwino ” ? 3 : 16 . Paulo ‘ anapemphela ndipo anasanjika manja ake pa io ndi kuwacilitsa . ’ ( 2 Maf . 12 : 4 , 5 ) Komanso , m’nthawi ya atumwi , abale atamva kuti anzawo akuvutika cifukwa ca njala , “ anatsimikiza mtima kutumiza thandizo lililonse limene akanatha kwa abale okhala ku Yudeya . ” — Mac . 11 : 27 - 30 . Mapangano amenewo amathandizanso atumiki ake kudziŵa kuti mbeu imeneyi ndiyo njila yokha yothetsela mavuto amene Satana anabweletsa pa mtundu wa anthu . GANIZILANI IZI : Muli ku malo osungilako zinthu zakale , ndipo kuli zoumba zakale - kale . 4 : 13 - 17 . Cifukwa cakuti Malemba amanena kuti mitundu yonse ya padziko lapansi , idzatengamo mbali pa kuukila komaliza kumene kudzayambitsa nkhondo ya Aramagedo . — Chiv . Tsiku laciŵili la utumiki wanga pa Beteli , n’nayamba kuseŵenzela m’fakitale yokonzela mabuku ku 117 Adams Street . Musakaikile kuti Yehova adzakuthandizani kupilila . — Ŵelengani Machitidwe 4 : 27 - 31 . Anali kudabwa kuti n’cifukwa ciani sapeza cimwemwe potumikila Mulungu ngakhale kuti amafuna kutelo . Ndiyeno , pogwila mau olembedwa ndi Mose , amene Asaduki anali kunena kuti anali kukhulupilila , Yesu anagwilitsila nchito mau amene Yehova anauza Mose pa citsamba coyaka moto . Mau amenewa anapeleka umboni woonjezeleka wakuti ciukililo ca padziko lapansi cidzacitikadi . — Eks . Ophunzila a Yesu sayenela kulalikila n’colinga copeza ndalama kapena kumanga nyumba zapamwamba . Mukalibe kusankha njila iliyonse , muyenela kufunsa ku ofesi ya nthambi kuti mudziŵe njila zimene n’zotheka m’dziko limene mukhala . ( b ) Tiphunzila ciani m’nkhani ino ? Mfumu Davide anauza Solomo kuti Yehova adzakhala naye mpaka pamene adzatsiliza kugwila nchito yomanga kacisi . Otsatila oyambilila a Yesu Khiristu , anali kudziŵika ndi dzina lakuti “ Akhiristu . ” Pamalo amenewa , anthu pafupifupi 6 mwezi uliwonse amapempha phunzilo la Baibo . Wina wake akakupatsani mphatso , mosakaikila mumaonetsa kuti ndinu oyamikila . “ ‘ Inu ndinu mboni zanga , ’ akutelo Yehova . ” — YES . Kodi Satana angatipangitse bwanji kuvula cisote cathu ? Iwo amanena kuti cimene cimapangitsa munthu kuganiza kuti pemphelo lake layankhidwa n’cakuti popemphela amakamba maganizo ake momasuka , amazindikila vuto lake , ndiponso amaganizila mmene angalithetsele . PA MBONI zacangu zimene zikutumikila ku malo kumene kuli ofalitsa Ufumu ocepa , ambili ni alongo amene ni mbeta . Tifunika kutsatila malangizo a m’Baibo amene akulu amatipatsa . Komanso , tidzakambilana mphatso zinayi zocokela kwa Yehova zimene zimatithandiza kupilila pogwila nchito imeneyi . Iye anatipatsa moyo . ▪ Kodi Yehova Waonetsa Bwanji Kuti Amatikonda ? Citsanzo ca Paulo cingatithandize bwanji pokonzekela ulaliki ? Koma popeza anali ocepa kwambili , io ayenela kuti sanali kudziŵa kuti adzakwanitsa bwanji kugwila nchitoyo . “ Imfa , mdani womalizila , idzaonongedwa . ” — 1 Akorinto 15 : 26 . CAKA COBADWA : 1974 Kodi Mumayamikila Zimene Munalandila ? Kodi buku la Levitiko lingatithandize bwanji ? MMENE BAIBULO INATETEZEKELA : M’cilamulo cimene Ayuda anapatsidwa , munali lamulo lakuti mfumu iliyonse iyenela “ kukopela buku lakelake la Cilamulo , ” kutanthauza mabuku asanu oyambilila a m’Baibulo . Ngakhale anthu amene satumikila Yehova amakamba kuti : “ Zoonadi Mulungu ali pakati panu . ” Panthawi ina , Yerusalemu anali mbali ya Ufumu waukulu wa Perisiya . Conco , tinakukila m’mudzi wina pafupi ndi mzinda wa Tallinn , ku Estonia , dziko limene linali mbali ya USSR . N’ciani cimasiyanitsa anthu ndi nyama ? Muyenela kudzifunsa kuti : Kodi pali njila yodalilika imene ndingadziŵile zamtsogolo ? Komabe , cofunika kwambili ndi mmene Yehova amationela osati mmene timadzionela , cifukwa iye amadziŵa zambili kutiposa . M’malo mogonja ku ziyeso zimenezi , kumbukilani zimene zinathandiza Yakobo , Rakele , ndi Yosefe kupitiliza kutumikila Yehova mwacimwemwe . N’ciani cinamupangitsa kuleka ? ( 1 Akor . 10 : 29 ) N’zoona kuti tili na ufulu wodzisankhila pa nkhani monga za maphunzilo na nchito . Koma tizikumbukila kuti ufulu wathu uli na malile , ndipo zosankha zathu zonse zimakhala na zotulukapo zake . Olo zili conco , m’mamaŵa amayenda pansi kupita ku malo opezeka anthu ambili m’tauni yawo , ndipo amafika kumeneko ku ma 07 : 00hrs . Koma kodi tifunika kuthela nthawi yoculuka bwanji pa zosangulutsa kuti zikhaledi zothandiza ? Zonse zimene Yehova amacita , amazicita cifukwa ca cikondi . Conco , iye afuna kuti olambila ake onse azionetsa cikondi , limene ni khalidwe lawo lalikulu . ( 1 Yoh . Iye anali kukhulupililabe “ Wosaonekayo , ” Yehova , ndi malonjezo ake . — Aheb . Koma , kumeneko n’nakhumudwa na khalidwe lonyansa la ciwelewele limene linali kucitika pakati pa ansembe na masisitele . Iwo anathamangila akananiwo ndi kuwapha ndipo sanasiyeko ngakhale mmodzi wa asilikali a Sisera . Zida izi zimafotokoza zambili ponena za malo , madeti a zocitika , kulemela kwa zinthu na kapimidwe kake , ndi zina zaconco . Nawonso akazi ayenela kugonjela umutu wa amuna awo . ( Aef . ( Salimo 68 : 5 ) Janet amadziŵa kuti Mulungu satiyesa ndi “ zinthu zoipa . ” Papita zaka zoposa 50 lomba . Madzulo pamene kunali kuomba kamphepo kayeziyezi , Samueli “ anapitiliza kulankhula ndi Sauli ali padenga la nyumba ” mpaka usiku pamene anapita kukagona . ( Miy . 15 : 30 ) Rachel , amene anasamukila kutali na kumene anakulila , anati : “ Mwacibadwa , ndine wamanyazi . Iye analemba Ezekieli 8 : 1 mpaka caputa 19 : 14 “ m’caka ca 6 ” ca ukapolo , kapena kuti mu 612 B.C.E . Pamene tinali ocimwa , Mulungu anapeleka Yesu kuti adzatifele cifukwa cotikonda ise mbadwa za Adamu . — wp17.6 , mape . Ndipo Davide analunjika kumutuko . — 1 Samueli 17 : 41 . Mau akuti “ kukonda abale ” amapezeka kwambili m’mabuku Acikristu . Pa nthawi ina , ndeke za nkhondo zouluka ca munsi zinaombela pa nyumba yathu pamene panali ine na ambuye anga aakazi . Anthuwo anayamba kudandaula cifukwa ca kusowa kwa madzi . 6 : 9 - 11 ) Ndi mmenenso Akhiristu a ku Roma nawonso anasinthila . ( Onani cithunzi pamwambapa . ) ( b ) Ndi kukhulupilika kotani komwe kwafala m’dzikoli ? Conco , dzifunseni kuti : ‘ Ngati mwininyumba wakambapo maganizo ake amene sagwilizana ndi zimene Baibulo imaphunzitsa , kapena ngati wafunsa mafunso ovuta , kodi nimakwanitsa kupeleka mayankho ocokela m’Baibulo ? 23 : 12 ) Ndinali kufuna kutumikila Mulungu amene amasamala kwambili za ife , cakuti anapeleka Mwana wake wamtengo wapatali monga dipo . Mose analola zocita za ena kumulepheletsa kuyang’anabe kwa Yehova . OLOŴETSEDWAMO : Yehova ndi Isiraeli wa kuuzimu N’tasiliza sukulu ya sekondale , n’napempha kuti nikatumikile kumalo osoŵa . Uzitsatila malamulo anga onse . Inde , “ cikondi sicitha . ” ( Mose asanapite ku Iguputo , Mulungu anam’phunzitsa mfundo yofunika kwambili . Pambuyo pake , Mose analemba mfundoyi m’buku la Yobu kuti : “ Kuopa Yehova ndiko nzelu . ” ( Yobu 14 : 14 , 15 ; Yoh . 5 : 28 , 29 ) Kuwonjezela apo , munthu wodzicepetsa amakumbukila kuti “ Mulungu woona adzaweluza nchito iliyonse ndiponso cinthu ciliconse cobisika , kuti aone ngati zili zabwino kapena zoipa . ” Adzagwilitsila nchito mphamvu zimene Atate wake anam’patsa kubwezeletsa anthu ku ungwilo . Iwo anali kuyesetsa kulambila Mulungu m’njila yoyenela , ngakhale kuti anali kupondelezedwa . Koma n’zomvetsa cisoni kuti anansi ake sanathawe . Tsanzilani Cikhulupililo Cao Cilimbikitso cimathandiza munthu kupitiliza kucita zabwino . Kukamba zoona , timafunika kukhala oganiza bwino pamene ticita cifunilo ca Mulungu ndiponso pamene tiyesetsa kukhala ndi cikumbumtima cabwino . Iwo ayenela kupewa kutengako mbali m’mikangano ya ndale , olo anthu ena andale aoneke kuti akucita zabwino kapena zacilungamo kusiyana ndi ena . Cakumayambililo kwa zaka za m’ma 1990 , zofalitsa zathu zinali za Cirasha , ndiponso misonkhano inali kucitika m’Cirasha . Ngati tilibe thandizo la mzimu woyela wa Mulungu , tingagonje ku “ nchito za mdima . ” N’cifukwa ciani nthawi zina tingafooke ngati timalalikila m’gawo la anthu opanda cidwi ? Buku imeneyi ipezekanso pa webusaiti ya www.jw.org . Onaninso “ Bokosi la Mafunso ” mu Utumiki Wathu wa Ufumu wa April 2011 , peji 2 . Paulo anaŵayamikila kwambili Akhiristu anzake m’makalata amene anawalembela . ( 1 Akorinto 10 : 23 , 24 ; Afilipi 3 : 17 ) Ngati tiganizila zimene Baibulo limakamba ndi zimene Yehova amafuna , tidzapanga zosankha zimene zidzam’kondweletsa . Kodi kuba kwa mtundu uliwonse Yehova amakuona bwanji ? Cifukwa ca zimenezi io amasiyanabe maganizo pankhani ya makhalidwe ndi ziphunzitso . Munthu amene wapha mnzake mwangozi akafika pacipata coloŵela mumzinda wothaŵilako , coyamba anali kufunika ‘ kufotokoza nkhani yake kwa akulu . ’ Ndimafuna kuonetsa kuti ndimayamikila mphatso ya moyo mwa kugwila nchito mwamphamvu kuti ndithandize ena . ” — David . 2 , 3 . ( a ) Kodi munthu amene ali na cikhulupililo adzalandila madalitso yabwanji ? Pambuyo pake ndinali kusinthanitsa nkhuku 50 ndi matumba aŵili a ufa olema makilogalamu 50 , ogulidwa pamtengo wa 110 paundi . M’masiku a mneneli Malaki , azimuna ambili aciyuda anali kucitila ciwembu azikazi awo mwa kuwasudzula pa zifukwa za mtundu uliwonse . Kosinthika Bwanji poneza za ife masiku ano ? Ndiye cifukwa cake Baibo imagogomeza kulimbikitsana nthawi zonse . Paulo anati : “ Posadziŵa cilungamo ca Mulungu , io sanagonjele cilungamoco koma anayesetsa kukhazikitsa cao - cao . ” N’cifukwa ciani sitiyenela kukayikila kuti ciukililo ca padziko lapansi cidzacitika mwadongosolo ? ( 2 Akor . 9 : 6 ) Mfundo ya pa lembali imagwilanso nchito kwa aja amene amaonjezela utumiki wao . Malinga ndi zimene ndafotokoza kale , mkazi wanga sindinali kum’patsa ulemu . Koma limakambanso kuti , “ Pa za malamulo , anthu amakhala na ufulu ngati m’dziko muli malamulo acilungamo , oyenelela , komanso osapondeleza . ” Maumboni aonetsa kuti kupatsa na cimwemwe kumagwilizana . N’cifukwa ciani Yehova anasankha Mariya kuti akhale mayi wa Yesu ? 15 : 30 ) Kodi nkhani ya Sauli ingatithandize bwanji monga galasi kuti tikhalebe ndi mzimu wodzimana ? ( Aheb . 11 : 27 ) Zina mwa zida zimenezo ni vidiyo yakuti The Wonders of Creation Reveal God’s Glory , kabuku kakuti Was Life Created ? ( 1 Mafumu 17 : 3 - 6 ) Ifenso tili ndi cikhulupililo cakuti Yehova adzatipatsa zimene tifunikila . Pamsonkhanowo , zilembo zakuti “ ADV ” ( zimene mau ake amatanthauza “ kulengeza ” m’Cizungu ) zinali kupezeka paliponse — pamitengo , pa zipupa za nyumba , ngakhalenso pa pulogilamu ya msonkhano . Potengela zimene anali kuona pa TV , m’magazini ndi m’manyuzipepala , iye anadziona monga ndi wotsogola . Munthu wopeleka mphatso moganizila ena sayembekezela kuti akamubwezele cifukwa ca kukoma mtima kwake . Zoona , Yehova Mulungu ndiye Wotisamalila wamkulu . Tsiku ndi tsiku anali kunyengelela Yosefe . Nikauka m’maŵa , mu mtima nimati , ‘ Kwaca lomba , niyende mu ulaliki ! ’ ” Komabe , lemba la Chivumbulutso limakamba za “ miyanda kuculukitsa ndi miyanda ” ya angelo . Kenako anaonanso ng’ombe zina 7 zonyansa ndi zowonda . Zocitika ngati zimenezi zingayese cikhulupililo cathu mwa Yehova ndipo zingapangitse kuti tizikayikila mmene gulu lake limayendetsela zinthu . Imodzi mwa njila zimene Paulo anaonetsela kuti anali kuyamikila nchito yolalikila , ndi kulalikila anthu pa mpata uliwonse umene wapezeka . Laura atalimbikitsidwa ndi zocitika zokondweletsa za mu ulaliki , anayamba kuganizila zosamukila ku mpingo wa cinenelo cina ku Canada . Yehova anali atauza Abulahamu kuti mtundu umene udzacokela mwa iye udzatsegula khomo la madalitso kwa anthu onse padziko lapansi . — Genesis 3 : 15 ; 12 : 2 , 3 , 6 , 7 . Iwo sadziŵa kuti cikhulupililo ceniceni n’ciani , kapena sadziŵa mmene cimagwilila nchito . Uthenga wabwino ukulalikidwa m’zinenelo zina 37 ndi ofalitsa oposa 24,000 . Coonadi ca m’Baibulo cikadzaza mumtima mwanu , mudzayamba kulakalaka kuuzako ana anu . Kudziŵa kuti Yehova ndi Gwelo la citonthozo ceni - ceni , kudzatithandiza kupilila mavuto aliwonse amene tingakumane nawo , lomba ndiponso mtsogolo . Ndinali kudziŵa malemba onse okhudza dipo ndiponso mmene ndingafotokozele malembawo . Nthawi imene iye anafika ku Taiwan kucita upainiya , kudelalo kunali mipingo iŵili cabe ya Cichaina , koma tsopano kuli mipingo 7 . N’ciani cocititsa cidwi tikaganizila madela amene kunali mizinda yothaŵilako mu Isiraeli na miseu yopita kumeneko ? Ngakhale n’conco , iye wapatsa atumiki ake mwayi wogwilitsila nchito cuma cawo pocilikiza nchito ya gulu lake . Iye analola kutsogoleledwa ndi Yehova popanga zosankha pa umoyo wake . PITILIZANI KUKULITSA CIKONDI CANU PA MULUNGU ( b ) Nanga odzozedwa aonetsa bwanji kuti ndi okonzeka ? Iwo anamwalila na zaka 93 . Conco , muziyamikila malo anu m’gulu la Yehova , ndipo ‘ muzimvela mau a Yehova Mulungu wanu . ’ Kodi mungakhale bwanji acimwemwe pa nchito yopanga ophunzila olo kuti mumalalikila m’gawo louma ? Ndinali kupitabe ku chechi nthawi zonse . Monga mmene Yesu anakambila , Mulungu “ adzaonetsetsa kuti cilungamo cacitika kwa io mwamsanga . ” — Luka 18 : 6 - 8 . Kwa zaka zambili , Kristu wakhala akukonzekeletsa mkwatibwi wake kaamba ka mwambo wa cikwati umene udzacitika kumwamba . ( Salimo 90 : 12 ) Inde , pemphani Yehova Mulungu mocokela pansi pa mtima kuti akuonetseni mmene ‘ mungaŵelengele masiku anu ’ mwanzelu , kuti nthawi yocepa imene yatsala kwa wodwalayo muiseŵenzetse m’njila yabwino koposa . 18 , 19 . ( a ) Ponena za kulambila koona , ndi mwai wotani umene Mulungu wapeleka kwa amuna ndi akazi ? Atumwiwo anamvetsela bwino - bwino pamene Yesu anali kuwaphunzitsa kulalikila mogwila mtima . Padziko lonse , oyang’anila madela aona kuti m’mipingo yambili akulu afunika kucita khama kuphunzitsa abale ena , acinyamata ndi acikule , kuti azisamalila gulu la nkhosa . Ngati m’bale wacinyamata akuonetsa kukula mwakuuzimu , ndipo ndi wodzicepetsa komanso akukwanilitsa ziyeneletso zina za m’Malemba , akulu angamuyamikile kuti aikidwe kukhala mtumiki wothandiza ngakhale kuti sanakwanitse zaka 20 zakubadwa . — 1 Tim . 3 : 8 - 10 , 12 ; onani Nsanja ya Olonda ya July 1 , 1989 , tsamba 29 . Ngati titsegula pakamwa mokwanila , tingathe kuimba mokweza . — w17.11 , peji 5 . Anthu a Yehova akale anali kunena mau amene ali pa Yesaya 64 : 8 akuti : “ Inu Yehova , inu ndinu Atate wathu . ” N’nali mmodzi wa twatsikana 4 tumene tunasankhidwa kuti tukapeleke maluŵa kwa Adolf Hitler atatsiliza kukamba ku gulu la anthu . 8 Tinamasulidwa mwa Cisomo ca Mulungu 19 Mbili Yanga — Yehova Sananigwilitse Mwala N’nali kudziona monga mwana wosiyidwa . N’takhala m’gulu , n’nacita cidwi kuona kuti Mboni zinali zaulemu kusiyana ndi anthu ocita phokoso amene n’nali kuona pocita maseŵela a baseball . Apo ayi , angayambe kugwilizana kwambili ndi acibale awo osakhulupilila , kapena anthu ocokela m’dziko lawo amene ali na cikhalidwe colingana na cawo . 36 : 9 ) Conco , mpake kuti Yesu anatiphunzitsa kupemphela kuti : “ Atate wathu wakumwamba . ” ( Mat . Nthawi zina ndimatopa kwambili , ndipo anthu sangadziŵe nchito imene ndagwila , koma ndimadziŵa kuti ndacita zinthu zofunika . ” Kudziŵa mmene Yehova anacitila zinthu ndi atumiki ake , amene anali ovutika maganizo , kungatithandizenso kusintha mmene timaonela ena . Ndikumbukila kuti anthu anacita zionetselo , ndipo anali kukamba kuti , ‘ Asilikali a ku America ndi opha ana . ’ ( Aheberi 11 : 1 ) Kuti tikhale na citsimikizo cimeneci tifunika kukhala na cidziŵitso colongosoka . Conco , pali pano tiyeni tiziyesetsa kupezeka pa Cikumbutso ciliconse . Komanso , tiziona mgwilizano umene timakhala nawo pa Cikumbutso kukhala wamtengo wapatali . Kumatithandiza kupewa zinthu zimene zingatitayitse ulemu , ndipo timalimbikitsa mgwilizano pakati pa anthu a Yehova . Ndithudi , kulanga kwabwino , ngakhale pamene tifunika kupeleka cilango , nthawi zonse kumacitika cifukwa ca cikondi . Paradaiso Padziko Lapansi — Ni Yeni - yeni Kapena ni Maloto Cabe ? 6 : 40 ) Zoona , ciyembekezo ca moyo wosatha ni mphatso yoonetsa kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . ( b ) Tidzakambilana ciani m’nkhani ino ndi yotsatila ? Daniel Molchan ( Yoh . 13 : 34 , 35 ; Aroma 5 : 6 - 8 ) Conco , m’malo mothetsa ubwenzi kapena kumupewa , dzifunseni kuti : ‘ Kodi zimene m’bale wanga amacita n’zosemphanadi ndi Malemba ? Cacikulu cimene Yehova anali kufuna pokamba na Yobu si kumufotokozela cifukwa cake anali kuvutika , ngati kuti Mulunguyo ndiye anacititsa mavuto ake , ndipo afuna kudzilungamitsa . Kodi Yesu anali kutanthauza kuti odzozedwa ambili adzakhala osakhulupika , ndi kuti adzafunika kuloŵedwa m’malo ndi ena ? Kodi Yehova anacita nkhanza mwa kupatsa Yobu uphungu wamphamvu pambuyo pakuti wapilila ciyeso cacikulu ? Nanga n’cifukwa ciani tiyenela kukhulupilila zimenezi ? Koma mtumwi Paulo anatumiziwa na mzimu woyela kuti akalalikile kwa anthu a mitundu ina , okhala m’madela olamulidwa na Aroma na Agiriki . Paulo anafotokoza kuti : “ Pakuti ngati ukulengeza kwa anthu ‘ mau amene ali m’kamwa mwakowo , ’ akuti Yesu ndiye Ambuye , ndipo mumtima mwako ukukhulupilila kuti Mulungu anamuukitsa kwa akufa , udzapulumuka . ( 1 Yohane 3 : 10 , 11 ) Mboni za Yehova zimadziŵika kuti ndi otsatila a Kristu oona cifukwa cakuti amakondana ndi kugwilizana . Ndipo Mulungu akuwagwilitsila nchito kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu padziko lonse . — Mateyu 24 : 14 . Mwa ici , anthu angafune kumvetsela uthenga wopatsa moyo umene tili nawo . Anacita zimenezo kuti omvela aone kuti anali kukamba zocokela kwa Yehova , osati za m’nzelu zake iyai . — Yoh . Ngakhale kuti Yesu anali wangwilo , iye anali wodzicepetsa ndipo anauza ophunzila ake kuti amadalila thandizo la Yehova . Ine na mkazi wanga , Tabitha , mu ulaliki Mwacitsanzo , ungatithandize kutengela makhalidwe a Yesu ndi kuonetsa makhalidwe amene mzimu woyela umatulutsa . Nanga bwanji ngati sakaniyankha bwino ? ’ M’nthawi zakale , asilikali anali kuzungulila mpanda wa mzinda kuti aulande . Antônio wa zaka 73 , wa ku Brazil , anakamba kuti : “ Ndimayesetsa kuti ndizioneka bwino ndipo ndimavala zovala zaudongo ndi zoyenela . ” Mipukutuyi yakhalapo kwa zaka zambili Katswili wa Cipangano Catsopano dzina lake Philip W . Komanso cifukwa cakuti Hava anamvela bodza la Satana , ndipo Adamu sanamvele Mulungu , ucimo ndi imfa zinafalikila kwa anthu onse . Conco , ndisanapeleke uphungu ndinaganiza zom’patsa mpata kuti akambe za kukhosi kwake . Kodi nthawi zina mumaona kuti miyezo yolungama ya Yehova ni yolemetsa kapena yovuta ? Acicepele , dzifunseni kuti : ‘ Kodi nimacita zinthu zauzimu cifukwa congofuna kukondweletsa makolo anga ? Vuto limeneli lingakucititseni kudziimba mlandu , cifukwa cakuti mumawakonda kwambili abululu anuwo , ndipo mwakhala mukuyesa - yesa kuwacitila zinthu zabwino . Pempho lathu n’lakuti mau ocokela pansi pa mtima okambidwa ndi abale na alongo otumikila ku Myanmar amenewa , akulimbikitseni kuyesetsa kuthandiza anthu oona mtima m’magawo osalalikilidwa . 25 : 8 ) Pambuyo pake , io anamanga kacisi wolambililamo Yehova . Iye wapitilizabe kucititsa kuti cifunilo cake cikwanilitsidwe Komanso mkulu wa opeleka cikho anali kuyang’anila atumiki a Farao amene anali kuonetsetsa kuti vinyo wopita kwa Farao unali wokoma ndiponso wosaipitsidwa ndi mankhwala amene angaphe mfumu . Kenako ŵelengani Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . Ena a iwo ni apainiya okhulupilika . Pa Kulambila kwa Pabanja , muzithandiza ana anu kumvetsa nkhani zimenezi n’colinga cakuti azicita zinthu molimba mtima akayesedwa kuti acite zimenezi . Koma zimenezi zinali ciyambi cabe ca zotulukapo zoipa za cosankha cake . N’zinthu ziti zimene Rose anasintha pa umoyo wake kuti akhale nzika ya Ufumu wa Mulungu ? Kudziletsa kumene mudzakhala nako kudzakuthandizani kukhala na umoyo wabwino , kukhala pa ubwenzi wabwino na Mulungu , ndi kukhala bwino ndi anthu amene mumawakonda . 1 - 3 . ( a ) Kodi lemba la Salimo 147 liyenela kuti linalembedwa liti ? Ponena za anthu akale a Mulungu , Baibulo limati : “ Makutu ako adzamva mau kumbuyo kwako , akuti , ‘ Njila ndi iyi . Iye anagwila mnyamatayo n’kumupsompsona . Yehova “ sadzalola kuti muyesedwe kufika pamene simungapilile ” ( 1 Akor . 10 : 13 ) , Feb . ( 1 Timoteyo 3 : 1 , 10 ) Akulu ena acinyamata , apita patsogolo kwambili mwakuuzimu . Ngati inde , pali masitepu amene angakuthandize kulimbilitsa cikhulupililo cako . Kodi mayankho a mafunso amenewa angatithandize kudziŵa mmene zinthu zidzakhalile mtsogolo ? Asayansi amene amafufuza za ukalamba amakhulupilila kuti angathe kutalikitsa moyo wa munthu . ( Sal . 37 : 25 ; Miy . Iye anati , anthu amene “ amadziŵa colinga ca moyo wawo , kaŵili - kaŵili amakhala na thanzi labwino . Iwo amapewa matenda a ubongo ndipo savutika kuphunzila na kumvetsa zinthu . . . . Amapewanso matenda a mtima , amacila mosavuta matenda a sitroko . . . , ndipo amakhalako na moyo wautali . ” Kodi pali cipembedzo cina cimene n’cofunitsitsa kutsatila kwambili Mau a Mulungu olo kuti kucita zimenezi kungabweletse mavuto kwa mamemba ake ena ? Yohane analimbikitsa Gayo kuonetsanso mzimu woceleza . Iye anauza Gayo kuti : “ Utsanzikane nawo [ Akhristu apaulendo ] m’njila imene Mulungu angasangalale nayo . ” Lemba la Salimo 45 limanena kuti coyamba Mfumu Yesu Kristu idzamangilila lupanga m’ciuno mwake ndi kugonjetsa adani ake . Ena anamasulila Malemba Aciheberi liu ndi liu , koma ena sanatelo . Cinayambila kwathu kweni - kweni , kumpoto kwa dziko la Kyrgyzstan . Tikunena pano , makope a bukuli oposa 200,000,000 asindikizidwa . Kodi Ufumu wa Mulungu Unayamba Liti Kulamulila ? — November - December 11 / 1 ( b ) N’ciani cingatithandize kuti tizilalikila momasuka uthenga wabwino ? “ N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kutsatira Mfundo za m’Baibulo ? ” — mutu 34 N’zoona kuti si aliyense m’mipingo ya m’delali amene amakwanitsa kuyenda misenga itali - itali kukalalikila . Iwo amathandizila kuti anthu oona mtima alandile uthenga wa m’Baibulo . Izi zimapeleka ulemelelo kwa Yehova ndi kum’sangalatsa . Patapita zaka ziŵili ndi hafu kucokela pamene kunacitika tsunami , io anagaŵila kapepala kauthenga ka mutu wakuti Kodi N’zoona Kuti Akufa Angakhalenso ndi Moyo ? 9 : 9 - 13 ) Kodi pamenepa tingakambe kuti Yesu anali kulekelela macimo ? Izi n’zimene zinacitikila m’bale wina dzina lake Federico . Anthu ena amaganiza conco . ( 1 Ates . 5 : 14 ) Ngakhale kuti abale na alongo ambili ofooka pambuyo pake amalimba m’cikhulupililo , ena timafunika kupitilizabe kuwathandiza moleza mtima . 1 : 28 ; Sal . 37 : 29 ) Mopanda kaso anapatsa Adamu ndi Hava mphatso zosiyana - siyana kuti asangalale ndi moyo . Kuti timvetse cifukwa cake Baibo ya Ciheberi ya Hutter inali yothandiza kwambili , ganizilani mavuto aŵili amene ophunzila analupeza poŵelenga Mabaibo ena a Ciheberi . N’nakulila m’tauni ya Puerto Limón ndi m’madela ena a kufupi ndi tauniyi . Gehazi analephela kuukitsa mwanayo . Panayiota anayamba kuphunzila Baibulo kenako anabatizidwa . Khalani Wolimba Mtima ndi Wozindikila Monga Yesu Kodi timalemekeza bwanji Yehova cifukwa ca kukoma mtima kwake kwakukulu ? ( Chiv . 17 : 12 - 14 ) Cikumbutso cimene cidzacitika odzozedwa atangotsala pang’ono kusonkhanitsidwa kupita kumwamba , n’cimene cidzakhala cothela . Zili conco cifukwa pa nthawiyo , Yesu adzakhala ‘ atafika . ’ Tikalakwa , timalapa moona mtima ndi kuleka kucita zinthu zosalemekeza Yehova . — Sal . Kodi mbalame zimafunikila eyapoti yotelapo ? 4 ‘ Pitilizani Kulimbikitsana Tsiku na Tsiku ’ Akatswili a zacipembedzo pa yunivesiti ya Sorbonne , mwamsanga anaŵelenga mosamala kwambili zimene Lefèvre anamasulila . Pamene nthawi ikuyenda , muzipatula nthawi yoonanso zimene mwacitako pofuna kukwanilitsa colinga canu . N’kutheka kuti iye anali kuganizila za tsogolo lake . Ngati sitisamala , tingalole kuti kusiyana kumeneko kuwononge mgwilizano pakati pathu . Kutulutsa Baibulo la Dziko Latsopano Lomasulira Malemba Achigiriki Achikhristu m’Cituvalu Mfundo imeneyi ikutionetsa kuti Yehova saona cinenelo kapena cikhalidwe cina kukhala cabwino kuposa cina . — Ŵelengani Machitidwe 10 : 34 . Nthawi zina ndimakagwilila nchito ku mabanki , koma m’malo mwa kuba m’mabanki amenewa ndine amene ndimawayeletsa . [ Mau okopa papeji 9 ] ( Mac . 1 : 8 ) Wophunzila akamacita zimenezi , m’pamene angadzipeleke zeni - zeni kwa Yehova m’pemphelo , ndipo pambuyo pake angalengeze poyela kudzipeleka kwakeko mwa kubatizika . Koma kodi mungacite ciani kuti muzisangalala pamene muŵelenga Baibo ? Mu 1991 , ine na mkazi wanga tinapezekapo pa msonkhano wacigawo woyamba umene unacitikila mu mzinda wa Alma - Ata , umene lomba umachedwa kuti Almaty ku Kazakhstan . Conco , angakuthandizeni kusankha moyo wabwino koposa . Pemphani Thandizo Kuti Mumvetsetse Baibulo 6 PETULO analila kwambili pambuyo pokana Yesu . Kenako anam’pangila tiyi . Pamene anali kucita zonsezi , anali kukamba naye nkhani za m’Baibo mwaubwenzi . Kufika panthawi imeneyi , John anayamba kusintha mmene anali kuonela a Mboni . Conco , anafunsa mafunso mlongoyo pa nkhani ziŵili zimene cikhulupililo cake ndi ca atate ake cinali kusiyana . Nthawi ndi nthawi , timakhala ndi zilakolako zoipa , kapena timavutika kuthetsa cofooka cinacake cimene tili naco . M’nthawi yovuta ino , Yesu Khristu amapeleka cilimbikitso na citsogozo kwa abale na alongo olefuka na opsinjika maganizo . Amacita izi kupitila mwa abale ake odzozedwa ndi “ akalonga , ” amene ni akulu a m’gulu la nkhosa zina . Kwa zaka mahandiledi kucokela pamene bukuli linalembedwa , anthu ambili anali kulidalila . Umboni wa zimenezi ni wakuti mipukutu 80 ya Cigiriki ya bukuli ikalipo , komanso pali mipukutu ya bukuli m’zitundu zina . 8 , 9 . ( a ) Kodi zinthu zinali bwanji kwa mkazi wamasiye wosauka ? Munthuyo anacita manyazi , ndipo anam’pepesa Luigi cifukwa comulalatila . Ndi mavuto otani amene okwatilana amakumana nao ? Mwina mukhoza kusintha zinthu zina ndi zina mu umoyo wanu kuti mukhale na nthawi yambili youzako ena coonadi ca mtengo wapatali . ( Aroma 12 : 18 ) Akamatsatila mfundo za m’Baibulo , amakhala ndi umoyo wacimwemwe . — Yesaya 48 : 18 . ( Akol . 2 : 20 - 23 ) Kuti Paulo awathandize kuteteza ubale wao wamtengo wapatali ndi Mulungu , anawalimbikitsa kuti : “ Ikani maganizo anu pa zinthu zakumwamba , osati pa zinthu zapadziko . ” Tingacite ciani kuti titumikile bwino Yehova ? Mungakonzekele bwanji kuti muzikapeza zofunikila pa umoyo pocita upainiya ? Ndipo ana amene anabadwamo anali vimphona vaciwawa , vochedwa anefili . ( Gen . 3 : 6 , 7 , 17 - 19 ) Popeza tikukhala m’dziko mmene muli anthu osayamikila , ifenso tingayambe kuiwala zinthu zabwino zimene Yehova waticitila . Cokumana naco canga coyambilila cinandiphunzitsa mmene kudalila maganizo aumunthu kulili kopanda nzelu . ( Sal . 32 : 8 ) Komanso makolo anu acikristu ndi akulu mumpingo angakuthandizeni kudziŵa mmene mungagwilitsile nchito mfundo zimenezo . Ndikakhala muutumiki , ndimayesetsa kutsanzila makhalidwe acikondi a Yehova ndipo maganizo anga olakwikawo anathelatu . ” Akucita ciani tsopano ? yopezeka m’Nsanja ya Olonda ya May 1 , 2008 . * Kuwonjezela apo , akatswili amakamba kuti tuzipangizo twa mtundu umenewu tumasintha zinthu zina mkati mwa cibalilo . Yehova afuna kuti atumiki ake amasiku ano aphunzitsidwe bwino kuti ayenelele kusenza maudindo m’gulu lake . Amosi anali kukhala m’mudzi wakutali . Ngakhale n’conco , iye anali kudziŵa miyambo ndi olamulila a m’nthawi yake . Malinga ndi zimene timaphunzila m’Baibulo , zinthu zidzacitika mwanjila yotsatilayi : Coyamba , “ hule lalikulu , ” kapena kuti Babulo Wamkulu , amene ndi ufumu wa dziko lonse wa cipembedzo conama lidzaonongedwa . ( b ) Kodi ndani anali m’gulu latsopano loyanjidwa ndi Mulungu ? Iye anati anthu angakhale ndi moyo wosatha kaamba ka cikondi ca Mulungu . Koma kodi tiyenela kucita ciani kuti tikapeze moyo ? 1 : 16 ) Popeza kuti Yehova amaonetsa kukoma mtima kwake kwakukulu m’njila zosiyana - siyana , timalandila madalitso ambili . Koma kodi tingatsimikize bwanji kuti kulambila koona kudzapitilizabe m’dziko lodzala na makhalidwe oipali ? ( Salimo 46 : 9 ) “ Pakuti oongoka mtima ndi amene adzakhale m’dziko lapansi , ndipo opanda colakwa ndi amene adzatsalemo . Kudzela mwa mzimuwu , Mulungu amapatsa munthuyo lonjezo la zinthu zamtsogolo , kapena kuti ‘ cikole ca colowa cake camtsogolo . ’ ( Genesis 1 : 27 , 28 ) Koma pambuyo pake , Adamu analeka kugwila nchito ndi Mulungu , ndipo zotsatilapo zake n’zakuti anakumana ndi mavuto amene anakhudza mbadwa zake zonse . — Genesis 3 : 17 - 19 , 23 . Pambuyo pake , anaonjezela dziko la Bangladesh kuti likhale mbali ya dela lathu . Baibo imati : “ Pamenepo Leviyo anasiya ciliconse , ndipo ananyamuka n’kumutsatila [ Yesu ] . ” 28 : 15 ; 2 Akor . 7 : 5 - 7 ) Ndiye cifukwa cake Paulo analimbikitsa Akristu kuti : “ Sonyezani kuti ndinu oyamikila . . . , mwa masalimo , nyimbo zotamanda Mulungu , ndi nyimbo zauzimu zogwila mtima . ” — Akol . 2 : 17 . NYIMBO 134 , 24 Kodi tingakambitsilane naye bwanji munthu amene amaganiza conco ? Iye sanacite kulengedwa ndipo panalibe cina ciliconse cimene cikanamlenga . Akulu mumpingo wa Stephen anati : “ Stephen ni m’bale wodekha , wakhama pa nchito , ndiponso wodzicepetsa . ” Kuti tifikile anthu ambili , tifunika kulalikila mwadongosolo ndiponso mogwilizana . Iwo anali kupita ku kacisi katatu pa caka kukapeleka nsembe kwa Mulungu wao , Yehova . Iye anasintha zocita zake mwa kucotsa mafano amene anaika . Anayambanso kutumikila Yehova mwakhama ndi kulimbikitsa anthu ake kutumikila Mulungu . ( b ) Timapindula bwanji tikamathandiza ofooka ? Monga mmene tionele , iye sanali kuona Goliyati ngati mmene Aisiraeli ena anali kumuonela . Kodi Yehova anamvela bwanji Yesu atabatizika ? Anapemphedwanso kucita nchito ya kalembela wa mpingo , kukamba nkhani za anthu onse ndi kuthandiza kukonzekeletsa misonkhano ikuluikulu komanso kuthandiza kumanga Nyumba za Ufumu . Tidzakambilana mafunso ati m’nkhani ino ? “ Upambane mu ulemelelo wako . ” — SAL . N’cifukwa ciani tifunika kucita khama mwa njila imeneyi ? ( Mat . 16 : 21 - 23 ; 26 : 31 - 35 , 75 ) Olo zinali conco , Yesu sanamukane Petulo , koma anamulimbikitsa na kumulamula kuti akalimbikitse Akhristu anzake . — Yoh . 21 : 16 . N’zimene zinatika kwa Toñi . Kodi inu pacanu mwaphunzila ciani m’nkhani ino ponena za kukhala munthu wauzimu ? Anthu ambili osakhulupilila anaphunzila coonadi pambuyo poona khalidwe labwino la mnzao wa m’cikwati amene anasintha ndi kutsatila zimene Mulungu amafuna . Amenewo ni anthu amene ‘ Mulungu woona analimbikitsa mitima yawo ’ kuti asiye nyumba zawo na mabizinesi awo . Kwa zaka pafupifupi 2,000 , Yehova wakhala akusankha amene adzakhale mafumu . 12 : 1 - 5 ) Samueli anapeleka citsanzo cabwino cimene ana ake Yoweli ndi Abiya , anali kufunika kutsatila . N’ciani cinathandiza Sheryl kupilila pamene ambili a m’banja lake anamwalila ? Conco , kuyambila mu December 1917 mpaka kuciyambi kwa 1918 , Ophunzila Baibo okwana masauzande angapo anagaŵila mwakhama mathirakiti 10,000,000 akuti , “ Kugwa kwa Babulo . ” Unali uthenga wolasa kumtima Machechi Acikhiristu . Ngakhale kuti mbali zina Ophunzila Baibo sanali kuzimvetsetsa bwino - bwino , mofanana na ise masiku ano , mfundo yakuti Baibo imaletsa kupha munthu anali kuidziŵa bwino lomwe . “ Natalie , mwana wathu wazaka 6 anatiuza kuti : ‘ Sindine ndaba mphete . Kuti mudziŵe zambili za lonjezo la Mulungu la moyo wosatha m’Paradaiso , onani nkhani 3 m’buku yakuti , Zimene Baibulo Ingatiphunzitse , yolembewa na Mboni za Yehova . Ndiponso , mukaŵelenga nkhani zoipa zokhudza ena , ganizilani amene angapindule ngati nkhaniyo yafalikila . Ganizilaninso cifukwa cake wina angafune kufalitsa nkhaniyo . Kusamalila anthu amenewa n’kovuta kwambili komanso n’kolemetsa . ( 1 Timoteyo 1 : 11 ) Na ise tingakhale na umoyo wacimwemwe ngati tiyesetsa kutengela makhalidwe a Mlengi wathu , maka - maka cikondi cake . M’nthawi ya Yesu , talente imodzi inali kulemela madinari pafupifupi 6,000 . M’pempheni kuti adalitse zoyesa - yesa zanu n’colinga cakuti zokambilana zanu na m’bale wanuyo zikayende bwino . Mau amenewa anali okwanila kuthandiza mwana wake wokondedwa wauzimu Gayo , kuzindikila kuti kalatayo inalembedwa ndi mtumwi Yohane . Komanso , anthu oipa ambili ayesa - yesa kuciwononga . ” Kodi Satana wacititsa bwanji “ khungu maganizo a anthu osakhulupilila ” ? Kucitila pamodzi zinthu za kuuzimu kumathandiza okwatilana kuyandikila Mulungu , ndi kukondana kwambili ( Onani ndime 5 , 6 ) Conco , madokota ena anayamba kumulondola kulikonse kumene wapita m’cipatalaco ali na nyeleti n’colinga cakuti amulase mankhwala otaitsa mimba . Pamene masinthidwe atikhudza mwacindunji , tiyeni tikhale odzicepetsa . Tiyang’ane pa cifunilo ca Yehova , osati pa cifunilo cathu . Don anakamba kuti Yehova angakhale mnzanga wapamtima , amene anganimvetsele paciliconse cimene ningapemphe panthawi iliyonse . ” Caka cotsatila pamene n’nakwanitsa zaka 19 , n’nakalembetsa monga munthu wokana kugwila nchito yocilikiza nkhondo cifukwa ca cikumbumtima cake . Ataika malilo , Ummi , mlongosi wake wa Peter , anauza Don kuti : “ Zaka ziŵili zapitazo n’nakambilana ndi Peter . 31 : 8 ; Sal . 9 : 9 , 10 ) Iye adzapitilizabe kutipatsa zonse zofunikila kuti tipitilize kumutumikila mokhulupilika . ( Yakobo 1 : 5 ) Mungaikidwe m’ndende kapena kulangidwa m’njila inayake cifukwa cokhala wokhulupilika kwa Yehova . Koma panthawiyi anacita chimo loopsa . Mwacitsanzo , pamene mu Isiraeli munali cilala cacikulu , Yehova anali kupatsa Eliya cakudya ndi madzi . Mau amenewa ananditsimikizila kuti n’zotheka kusintha . Tiyamikila Yehova , Mulungu wa mtendele cifukwa cakuti amatipatsa zilizonse zofunikila kuti ticite cifunilo cake . ( Oweruza 4 : 9 ) Kodi kulimba mtima kwa Debora ndi amuna amenewa kukutiphunzitsa ciani ponena za cikhulupililo ? Mwanjila imeneyi ndiponso m’njila zina zosiyana - siyana , n’naona kuti Yehova ananisamalila mwacikondi . Hananiya na Safira analephela kucita zimenezi . Kumbukilani kuti Yesu anati : “ Pakamwa pamalankhula zosefukila mumtima . ” Koma pamene anafika ku Pamfuliya , mwadzidzidzi Maliko anawathaŵa . Iye anati : “ Pamene mpingo wathu unagaŵidwa , ndinapatsidwa maudindo oonjezeleka monga mtumiki wothandiza . Koma mofulumila mtsikanayo anayankha mwanzelu ndipo analimbikitsa atate ake kuti akwanilitse lonjezo lao kwa Yehova . Nayenso Gianni anati : “ Maurizio ndiye anali woyamba kuniphunzitsa Baibo . Koma pamene makolo anga anaphunzila zizindikilo za maso ake , anali kumupatsa zimene akufuna ndipo nkhope ya Jairo inali kukondwela kwambili . ( Ŵelengani Akolose 3 : 13 . ) N’cifukwa ciani n’zotheka kwa mwamuna ndi mkazi kukhala m’cikondi ceniceni ? Ganizilani cabe mmene timapindulila cifukwa comvela malamulo a m’Baibo oletsa kunama , kucita cinyengo , kuba , ciwelewele , ciwawa , na zamizimu . Koma adzalandila yankho lofanana ndi limene anthu ambili amene ali ngati mbuzi adzalandila panthawi yaciweluzo . Iye adzati : “ Kunena zoona , sindikukudziŵani inu . ” N’ciani cimakucititsani cidwi mukaganizila mmene Yesu anali kugwilitsila nchito mphamvu zake zozizwitsa ? Onetsetsani kuti kutumikila Yehova n’kofunika kwambili pa umoyo wanu Anthu odzipeleka ndi amene amagwila nchito yopanga mapulani a nyumbazi , kumanga , ndi kukonzanso zimene zaonongeka . Kudzikayikila : Kodi mumafuna kukhala oceleza , koma mumadzikayikila ? Iyai , umabala mbewu yatsopano , imene m’kupita kwa nthawi , nayonso imakula n’kukhala mmela wa tiligu . Ngati n’conco , mucita bwino . ( Aefeso 6 : 10 - 12 ) Macenjezo amenewa timawapeza m’Baibulo ndi m’mabuku amene gulu la Yehova limafalitsa . Nthawi zambili , tinali kuitana abale a citsanzo cabwino kunyumba kwathu , amene anali kulimbikitsa ana athu mwauzimu . Titatsiliza maphunzilo ine na Bethel tinatumidwa ku Nairobi , ku dziko la Kenya . Palibe aliyense angalimbane na Yehova . Mkuluyo anabwelezanso zimene anakamba , ndipo Fernando anaonetsa kukondwela pankhope yake . Motelo , anacha Paulo kuti Heme ndipo Baranaba anamucha kuti Zeu . Ngakhale kuti wopelekela cikho uja anamuiŵala Yosefe , Yehova sanamuiŵale . Koma mavuto onse amene timakumana nawo akadzatha , tidzakondwela ngako . Ngati Mkristu wanena kuti ndi wodzozedwa , kodi ena amene ali ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi ayenela kucita ciani ? Nimaona kuti zonsezo zinali kunikonzekeletsa maudindo a kutsogolo . Pokhala m’phunzitsi wa ana m’cipembedzo cao , io anali kukhulupilila kuti imfa si mapeto a zonse . Kapena atamupempha nsomba , kodi angamupatse njoka ? M’ma 1940 , Boma la Nazi linam’tumiza ku ndende yozunzilako anthu . Pambuyo pa zaka zingapo , boma la Soviet Union linam’tumiza ku dziko lina lakutali , kukakhala monga mkaidi . Nthawi zambili polalikila khomo ndi khomo , timapeza kuti anthu acokapo panyumba . Kodi Mulungu anacita ciani m’nthawi zakale ? Nanga anthu ena masiku ano amaganiza ciani akadwala ? ( b ) Nanga malangizo a Yehova tiyenela kuwaona bwanji ? Ndi mwai wapadela kuti Yehova wapempha anthu opanda ungwilo kukhala anchito anzake . ( 1 Akor . Pamene n’nali ndi zaka 16 , dziko la Britain linayamba kumenya nkhondo ndi dziko la Germany mu September 1939 . Ngati yankho n’lakuti ayi pa funso imodzi kapena onse aŵiliwa , mwina zingakhale bwino kuti udindo watsopanowo upite kwa munthu wina amene angausamalile bwino . Kodi Mumaona Dzanja la Mulungu pa Umoyo Wanu ? Iye anandiuza kuti , ‘ Musadandaule Atate . Ofalitsa 10 osamva mu mzindawo anakondwela ngako kuti anthu 62 anapezeka pa Cikumbutso mu 2015 Koma ndife ogwilizana polambila Yehova . Nowa anafunika kukhulupilila Yehova kuti adzasunga lonjezo lake la kucotsa zoipa zonse , ndi kuti adzacita zimenezo panthawi yake . — Gen . Mwacitsanzo , munthu amene ni katswili wolosela zam’tsogolo , amafunsa mafunso osiyana - siyana na kuyang’anitsitsa pamene munthuyo akamba na zizindikilo zinazake zimene aonetsa . 104 : 24 ; Chiv . 4 : 11 ) Conco n’kupanda nzelu kuganiza kuti zimene ife timacita ndiye zabwino kuposa zimene ena amacita . Inde , kukhala ozindikila na oganizila ena kungathandize onse kuti azilalikila uthenga wabwino modzipeleka , kaya ni acicepele kapena acikulile , aciyambakale kapena acatsopano . — Lev . Conco , alambili oona saika dala moyo wawo paciswe poganiza kuti angelo a Mulungu adzawateteza . Wamasalimo Davide anaimba kuti : “ Ndidzakukondani inu Yehova , mphamvu yanga . ” ( Sal . Tingaonetse kuti timayamikila Mulungu pa zinthu zabwino zimene watipatsa mwa kuika zinthu za Ufumu patsogolo paumoyo wathu . Tsopano ndinali wokonzeka kuphunzila Baibulo ndi alongo aŵili aja , Ilse ndi Elfriede . Ndithudi , uthenga wathu udzakhala ngati mame amene amadontha pang’onopang’ono , amatsitsimula , ndipo ndi ofunika kwambili pa moyo . ( Chivumbulutso 12 : 10 ) Ngakhale lelolino , Satana akali kukamba kuti anthu amatumikila Mulungu cifukwa ca dyela . Nayenso , Julian amene wakhala akudwala matenda opha ziwalo kwa zaka 30 , amamvela cimodzimodzi . Masiku ano , anthu mamiliyoni ambili padziko lonse akulambila Yehova . Monga takambila kale , kucilikiza ulamulilo wa Yehova ndiyo nkhani yaikulu yokhudza anthu onse . Mwamunayo waona kuti iye ndi mkazi wake sakhala na nthawi yokwanila yoceza , ndipo afuna kuti iwo acitileko pamodzi zinthu zina monga banja . Muziyelekezela zimene mwamva ndi “ citsanzo ca mau olondola ” ca m’Baibulo Coyamba , nkhani ya Sauli itiphunzitsa kuti ngati tili ndi mzimu wodzimana sitiyenela kukhutila ndi kuganiza kuti tidzapitilizabe kukhala nao . ( 1 Tim . Ndi mapindu otani amene wapezeka cifukwa cokhala Mkristu ? Ndi acibale angati amene Nowa anathandiza kukhala alambili a Yehova ? Mwina Luka , amene anali dokota , ndi amene anayambila kufika pamene Utiko anagwela . Iye atamuona , anakamba kuti Utiko sanavulale cabe kapena kukomoka , koma wafa . Tiyeni tikambilane mfundo zitatu zofunika zimene zingatithandize kukulitsa cikondi cathu pa Yehova . ( 1 ) Atate wathu amatipatsa zinthu zabwino . Posakhalitsa , Lauri ndi Ramoni nawonso anacoka . Iye zimam’pweteka kwambili akaona kuti anthufe tikukumana ndi mavuto osiyanasiyana , komanso kuti tili ndi moyo waufupi . — Ŵelengani Yobu 14 : 1 , 14 , 15 . Msonkhano umenewo unali wa mutu wakuti “ Ufumu Wolakika . ” Ndiye mungafunse kuti : ‘ Ngati Baibo ni yothandizadi , kodi thandizo lake silifunikila kuonekela mu umoyo wanga ? Kalata ya mtumwiyu inalembedwa ca m’ma 98 C.E . , ndipo m’Malemba Acigiriki Acikhristu , imachedwa “ Kalata Yacitatu ya Yohane . ” Nkhani ya m’Baibulo imeneyi , yathandiza abale ndi alongo ambili masiku ano kukhala olimba mtima ndi kukana kulambila mbendela ya dziko lao . ( Maliko 9 : 24 ) Monga atumwi , tingakambenso kuti : “ Tionjezeleni cikhulupililo . ” — Luka 17 : 5 . Kenako Davide anafika pafupi , ndi kutenga lupanga la Goliyati n’kumudula mutu . — 1 Samueli 17 : 48 - 51 . Mukuyembekezela kudzasangalala ndi mtendele woculuka pamodzi ndi banja lanu ndi anthu ena olungama . Ana anakamba kuti : “ Ndinakhuthulila Yehova nkhawa zanga zonse ndi kumucondelela kuti andithandize kupilila cisoni cacikulu cimene ndinali naco . ” Kukhala okhulupilika kwa Yehova kumafuna kucita zinthu molimba mtima anthu akatiopseza ( Onani ndime 15 ndi 16 ) Kaya colinga ca Mdyelekezi cinali cotani , Mikayeli molimba mtima anam’kaniza Mdyelekezi . 14 , 15 . ( a ) N’ciani cionetsa kuti Yehova amalakalaka kuthetsa mavuto onse a anthu ? Iye anali atangobatizika kumene kukhala wa Mboni za Yehova , ndipo anali na zaka 20 cabe . Panthawi imeneyo Atate anatumiza ine ndi mkulu wanga ku sukulu ya Ciyuda . Nanga tingacite ciani kuti Yehova aticitile cifundo na kutikhululukila ? Anthu a Yehova amayamikila kukhala ndi okalamba mumpingo . Koma sanali cabe wolimba ndi wokongola . Ndi Mboni za Yehova zokha zimene zikugwila nchito yocititsa cidwi imeneyi . 49 : 1 - 3 ) Ndakhala ndikuona cimwemwe cimene anthu amakhala naco akalandila cofalitsa catsopano m’cinenelo cao , kapena akamaimba nyimbo zotamanda Yehova m’cinenelo cao . Timaŵelenga kuti : “ Abulahamu anaipidwa nazo kwambili zimenezi cifukwa ca mwana wake . ” Timadziŵa bwanji kuti Yesu adzabwela pa cisautso cacikulu kudzaŵelengela cuma cake ? Nafenso timafunika kupanga zosankha . Mwacitsanzo , pamene Gidiyoni anasankhidwa kuti alanditse anthu a Mulungu amene anali kupondelezedwa ndi Amidyani , ayenela kuti anadabwa ndi moni umene mngelo anam’patsa kuti : “ Yehova ali ndi iwe , munthu wolimba mtima ndi wamphamvuwe . ” Mu 1916 , M’bale Russell anali ndi cidalilo cakuti uthenga wabwino udzalalikidwa padziko lonse lapansi . Kodi Christopher amene wachulidwa kuciyambi kwa nkhani ino , amamva bwanji cifukwa cosankha kubatizidwa ali ndi zaka 12 ? 1 , 2 . ( a ) Kodi mboni ya Yehova yopambana onse ndani ? Ndiyang’ana mtsogolo kudzaona anthu akuukitsidwa padziko ndili kumwamba , ndi kudzaonanso atate wanga a kuthupi N’cifukwa ciani anthu ambili amene anamva Yesu akulankhula analephela kumvetsetsa tanthauzo la zimene iye anali kukamba ? Kukambilana Ndi Munthu Wina Nkhani za m’Baibulo Paulo anali kulalikila mwakwama , ndipo anasiya citsanzo cabwino kwa Akhiristu masiku ano . Anaonetsadi kuti kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu “ sikunapite pacabe . ” Ndipo m’mwezi wina ninakwanitsa kutsogoza maphunzilo a Baibulo 24 . Pamene ndinali kutuluka m ’ Nyumba ya Ufumu , m’bale wina wa zaka pafupifupi 80 anandiimitsa . Zinthu zopanda cilungamo ngati zimenezi zimakhumudwitsa . Koma pali zinthu zina zopanda cilungamo zimene Akhristu angaone kuti n’zovuta kwambili kuzipilila . Conco , iye anali mtumiki wamkulu koposa komanso wodalilika wa Abulahamu . Yehova amalola mbeu za coonadi kukula mwa munthu yekhayo amene ali ndi mtima wodzicepetsa ndi wofunitsitsa kusintha . ( Mat . ( Mlal . 5 : 6 ) Conco , tiyeni ‘ tiziyimba mokondwela nyimbo zotamanda dzina la Yehova mpaka muyaya , pamene tikukwanilitsa malonjezo athu tsiku ndi tsiku . ’ — Sal . Maloto amenewo anali ocokela kwa Yehova Mulungu . * Zikomo kwambili cifukwa ca khama lanu . Ena mwa anthu aconco timaseŵenza nawo , kuphunzila nawo ku sukulu , kapena kukhala nawo . Nthawi zina , munthu angakhale na cisoni cacikulu , koma osakwanitsa kufotokoza mmene akumvelela . Ine na anthu ena tinayenda ulendo wa makilomita 8 kupita ku nyumba kwa m’bale Cruz , kumene kunali kucitikila msonkhano . Cina , tifunika kumvela malangizo amene Akhiristu ofikapo kuuzimu angatipatse . N’kutheka kuti Merozi unali mzinda umene nzika zake sizinafune kudzipeleka kukathandiza Aisiraeli pankhondo . Olo kuti n’nali na zaka 17 cabe , anatipatsa udindo pamodzi na mnzanga wocititsa misonkhano . Zinali conco cifukwa abale apaudindo anali ocepa mumpingo watsopanowo . M’nkhani yotsatila tidzakambilana mfundo zothandiza . [ Mau apansi ] Caka cotsatila asilikali aciroma anapitanso kukagonjetsa mzinda wa Yudeya motsogoleledwa na Kazembe wa nkhondo dzina lake Vespasian na mwana wake Tito . Masiku ano , gulaye angaoneke ngati cida cosathandiza , koma kale cinali cida coopsa kwambili . Yehova anacititsa Debora kulimbikitsa ndi kutsogolela woweluza Baraki , munthu wa cikhulupililo , kukamenyana ndi Sisera . — Oweruza 4 : 3 , 6 , 7 ; 5 : 7 . Wamasalimo Davide anati : “ Wolungama akandimenya ndiye kuti wandisonyeza kukoma mtima kosatha , ndipo akandidzudzula ndiye kuti wandidzoza mafuta pamutu panga . ” ( Sal . Mwacitsanzo , nthawi ina anayamikila msilikali wina cifukwa ca cikhulupililo cake cacikulu . Zidzaoneka ngati kuti anthu a Yehova ndi osatetezeka , koma kuukila anthuwo kudzaputa mkwiyo wa Mulungu . — Ezek . Iye anali wothela pa ana 8 aamuna . Mwacitsanzo , limakamba za mmene mngelo Gabirieli anaonekela kwa Mariya , za ulendo wa Mariya wokaceza kwa m’bale wake Elizabeti , na zimene Mariyayo anakamba potamanda Yehova . Ngati ticita zinthu mogwilizana ndi amene akutitsogolela , timaonetsa kuti tikucilikiza ulamulilo wa Yehova . Mofanana ndi Ulf amene tam’chula kuciyambi , nthawi zina tingakumane na mayeselo okhalitsa , cakuti sitingacitile mwina koma kuwapilila . Pamene Yesu anali kupita ku Samariya , anaimilila pa citsime pafupi ndi mzinda wa Sukari kuti apumule . Cyril analeka nchito , ndipo mwezi ukalibe kusila onse anayamba upainiya . Kodi Petulo anaonetsa bwanji kuti anali ndi mtima wodzikonda ? Yehova walonjeza kuti adzakhala ndi atumiki ake . Monga mmene makolo athu anacitila , tinacita zomwe tingathe kuti tizipezeka pamisonkhano ndi muulaliki nthawi zonse monga banja . Pilato anali munthu wosamva za ena . ( 2 Akor . 6 : 1 ) Anthu masauzande ambili akali mu ukapolo ku cipembedzo conama . Tapeza mabwenzi ambili , ndipo sitisoŵa kanthu kalikonse . Iye anakamba za malemba amene sin’nali kuwadziŵa bwino . ( b ) Kodi zofalitsa zathu zimafotokoza kwambili pa ciani masiku ano ? ( Gen . 19 : 14 ) Loti yekha ndi ana ake aakazi amene anagwilizana naye kwambili ndi amene anapulumuka . ( 1 Sam . 24 : 4 - 7 ; 26 : 8 - 12 ) Pamene Sauli anafa pa nkhondo , Davide anamulila . M’nkhani ziŵili zimenezi , tiphunzila cifukwa cake tingakambe kuti Yehova ni “ wotiumba . ” Tiphunzilanso zimene tiyenela kucita kuti tikhale ngati dothi lofewa m’manja mwa Yehova . Cotelo simukufunikila wina aliyense kuti azikuphunzitsani , koma popeza kuti munadzozedwadi moona osati monama , cifukwa ca kudzozedwako , mukuphunzitsidwa zinthu zonse . Anthu oposa 2,000,000 anafa ndi njala ku Russia mu 1921 . Patapita nthawi yocepa , ku madela ena kunagwanso njala . Mkambi ameneyo anati : “ Ganizilani citsanzo ici : Munthu angathe kukhotetsa galimoto kuti ipite kudzanja lamanja kapena lamanzele pokhapo ngati galimotoyo iyenda . Ndi cimodzimodzinso ndi utumiki wathu . Kukhala ndi maganizo oyenela kumatanthauza kukhala wofunitsitsa kuvomeleza mfundo zosiyanasiyana zatsopano . Koma kodi Davide anali kufuna kuti Yehova amucilitse mozizwitsa ? Takamba zimenezi cifukwa anthu 10,000 ocokela m’madela ozungulila Merozi anasonkhana kuti akamenye nkhondoyo . Ndipo patsikulo , abale ndi alongo anu anali okondwa kwambili poona kuti mumakonda Mulungu ndi mtima wanu wonse , moyo wanu wonse , maganizo anu onse , ndi mphamvu zanu zonse . — Maliko 12 : 30 . ( Miy . 3 : 27 ) Nthawi zambili alongo amaona zambili kupambana abale . Amai ndi ambuye ake a mnzakeyo anamulandila bwino ndipo anamufunsa mafunso ambili okhudza zikhululupililo zake ndi nchito yake monga mlaliki wa nthawi zonse . Khalidwe lake ndi mtima wake . N’zoona kuti kuseŵenzetsa cida ciliconse podziteteza kungapangitse munthu kukhala na mlandu wa magazi . Komabe , kukhala na mfuti kungapangitse munthu kupha wina mosavuta , kaya mwangozi kapena mwadala . Motelo , mungakhalebe olimba kuuzimu kaya muli ndi Intaneti kapena ai . Ngakhale kuti io anatelo , ine ndinayesetsa kuti ndipezenso Mboni za Yehova kuti ziyambe kundiphunzitsa Baibulo . Conco , mu July 1953 , n’nakwela boti yochedwa Georgic kuyenda ku New York , ku America . M’bale wina wa ku Canada anafotokoza kuti pa nthawi ina anali kuzonda kwambili anthu okamba zitundu zina . A Zimba : Ndikumvetsa zimene mukunena . ( a ) Kodi ubwenzi n’ciani ? Mankhwala amene John anali kumwa a khansa anali kumucititsa kuti azikhala otopa ndi kumva mseru . Kodi kudziŵa Mulungu molondola kunam’thandiza bwanji Nowa ? Tikadwala , timafunafuna njila zodzithandizila kuti tipole . Kukonda Yehova kuyenela kutilimbikitsa kutaya kapena kucotsa zinthu zonse zosayenela kwa Mkristu , ngakhale zitakhala zodula . Kucita zimenezi kungamuthandize kukhala wokonzeka kumvetsela malangizo amene mudzamupatse . — 1 Tim . N’zocitika ziti zimene zinayesa kukhulupilika kwa Aisiraeli ? Asanamwalile , iye anapeleka zinthu zoculuka kwa ana ake aamuna ambili . Kuti ticite zimenezi tingafunike kukambilana naye maulendo angapo . Zimenezi zimatilimbikitsa kum’khulupilila ndi kumumvela . Kodi Mulungu Analenga Mdyerekezi ? Mfundo imodzi yofunika kwambili ndi imene imapezeka pa Aheberi 13 : 1 , pamene pamati : “ Mupitilize kukonda abale . ” Yesu amatifunila zabwino , ndiye cifukwa cake anatiphunzitsa kuti tiyenela kufuna - funa Ufumu coyamba osati zinthu zakuthupi . Kucoka nthawi imeneyo , ndinadziŵa kuti Mboni za Yehova zimakwanilitsa mau a Yesu a pa Yohane 13 : 35 , akuti : “ Mwakutelo , onse adzadziŵa kuti ndinu ophunzila anga , ngati mukukondana . ” Mukumva bwanji tsopano ponena za buku la m’Baibulo la Levitiko ? Tinaona Cisomo ca Mulungu m’Njila Zambili ( D . Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Mwakutelo , onse adzadziŵa kuti ndinu ophunzila anga , ngati mukukondana . ” ( Yoh . ( 1 Akorinto 10 : 14 ; 1 Yohane 5 : 21 ) Conco , Akristu oona sayenela kulambila Mulungu pamalo amene anthu amaona kuti ndi opatulika kapena amene amalimbikitsa kupembedza mafano . Nawonso afunika kuwaonetsa njila yocokelamo , ndipo ise tingawalongoze njilayo . Kumbukilaninso kuti tikhoza kufikila “ Wakumva pemphelo , ” tili na cidalilo cakuti adzamvetsela mavuto athu . Conco , pamene Yehova anapatsa Adamu na Hava lamulo , anali kuwaphunzitsa njila yokhalila na ufulu weni - weni . Malinga ngati nthambi n’zolumikizika kumtengo wa mpesawo , zimalandila madzi na cakudya kucokela kumtengowo . Iwo anaphunzitsidwa za Yehova na atate awo kuyambila ali ana , ndipo anabatizika ali acicepele . Panalibe mabasi kapena mataksi amene anali kufika ku madela amenewo . Conco , tisamacite mantha kapena kucita manyazi kuimba . kwa Davide ? Koma monga taonela m’citsanzo ca Mfumu , ngati tayamba kudzikudza , tidzadzipeza m’mavuto aakulu ndi Mulungu . Kodi M’bale Russell anakamba ciani ponena za nchito yolalikila ? Nanga zimenezo zakwanilitsidwa bwanji ? Ganizilani citsanzo ca Uwe . Ngakhale kuti anayesetsa kuti akambe mmene anali kumvela , anali kungotulutsa mau omvekela kukhosi . Zimenezi zikadzacitika kwa inu musakagonje . Katherine atasamukila ku mpingo watsopano , anayamba kuphunzila Baibulo ndi Doris , mkazi wa zaka za m’ma 40 . Zingangotanthauza kuti sacedwa kugwila zinthu . Kucokela ca m’ma 1875 , amuna ndi akazi ocepa anali ndi cidwi pa kulambila koona . N’zoona kuti zinthu zina zimene zakhala zikucitika m’dziko zatithandiza kulalikila mosavuta . Koma timanzuzidwabe ndipo timakumana ndi mavuto ambili cifukwa ca dziko la Satana . Zakhala zotheka kulalikila cifukwa ca thandizo la Yehova . — Yes . Baibulo limati : “ Cikhulupililo copanda nchito zake ndi cakufa . ” Makolo a mnzanga anali a Mboni za Yehova . Fanizo la Yesu la nkhosa ndi mbuzi limatiphunzitsa kuti amene ali ndi ciyembekezo ca padziko lapansi ali ndi mwai wocilikiza abale odzozedwa a Yesu mokhulupilika panchito yolalikila ndi kuphunzitsa . Nthawi na nthawi , kamvedwe kathu ka maulosi a m’Baibo kapena Malemba ena kamasintha . Zofanana ndi zimenezi zikhoza kuticitikila masiku ano . N’nakumbukila kuti Baibulo imakamba kuti “ zinthu zosayembekezeleka ” zingathe kugwela aliyense wa ife . Katswili wina dzina lake D . Anthu ena anali kudana ndi uthenga wathu , moti akatenga khadilo anali kungoling’amba . Iye sanali kucitako macimo aakulu ochulidwa pa 1 Akorinto 6 : 9 - 11 . Tiyenela kuyesetsa kutengela zitsanzo za Akhristu okhulupilika amenewa , pamene nawonso akutsatila Khristu . — 1 Akor . Tikadalila Yehova ndi kupewa kufuna - funa zinthu zilibe phindu kapena kugula zinthu zilizonse zimene taona , Yehova adzakhala bwenzi lathu lapamtima . Iwo anayamba kugulitsa zakudya kuti azisamalila ana ao anai . Ndinali kufuna kupeputsila mwamuna wanga mtola ndi kugulila mwana wathu Jimmy zinthu zimene anzake ku sukulu anali nazo . ” Kenako , mukuzindikila kuti ngati simucoka pakati pamseupo , mugundidwa ndi basiyo . Koma mfundo yake imagwilanso nchito kwa amuna acikhiristu . Atumiki a Yehova afunika kuvala moyenelela . COCITIKA 15 : 28 , 29 ) Tikapsinjika maganizo , “ mitima yathu ingatitsutse . ” Ndipo sindinamvepo kuti ndili pafupi naye . ” Muyenela kukhala ololela kuti mwana wanu adzasintha , koma panthawi imodzimodzi , simuyenela kulekelela khalidwe loipa la ana anu . Adamu womalizila anakhala mzimu wopatsa moyo . ” — 1 Akor . Zaka zambili m’mbuyomo , Asuri ndiponso pambuyo pake Ababulo anali atatenga Ayuda kupita nao ku ukapolo . ( 1 Tim . 3 : 1 - 13 ; Tito 1 : 5 - 9 ) Kodi mipingo inapindula bwanji potsatila malangizo ocokela ku bungwe lolamulila ? Masiku ano , Satana akuukila kwambili mabanja . Baibo imaticenjeza kuti sitiyenela kungotsatila mtima wathu kapena kucita zinthu mongotengeka popanga zosankha . * Tsiku lina , mwamuna wolandila alendo mu hotelo , anandiitana ndi kundiuza kuti kuli azimai aŵili m’galimoto amene anali kufuna kundiona . ( Agal . 2 : 9 ) Mofananamo , mwamuna amene kale anali mkulu angayambenso kutumikila ndi kupezanso cimwemwe polimbikitsa okhulupilila anzake mwa kuuzimu . Ni Ufumu wa Mulungu cabe umene udzacotsapo kupondeleza ndi kupanda cilungamo na kubweletsa mpumulo weni - weni . — Mlal . Zimenezi zinaonetsa mmene anthu a Mulungu anamasulidwila ku ukapolo wa Babulo Wamkulu mu 1919 . Onani buku yakuti ‘ Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu , ’ mapeji 58 - 59 . Angagwilitsile nchito angelo ake kuti atithandize . — Aheb . TIKUKHALA ‘ m’nthawi yapadela komanso yovuta . ’ Posacedwa , mitundu yonse ya anthu idzakumana ndi cisautso cacikulu , cimene sicinacitikepo padzikoli . ( Mat . Koma kodi zimenezi zitanthauza kuti munthu aliyense , cocitika ciliconse , ndi cinthu ciliconse cofotokozedwa m’Baibulo , zimaimila winawake kapena cinacake ? Tingadziŵe bwanji ngati cikhulupililo cathu cayamba kufooka ? Koma bwanji ngati pali pano io ayamba kukaikila coonadi ? Athandizeni kumvetsetsa kuti kutumikila Yehova ndi njila yabwino koposa , ndipo kumabweletsa mapindu osatha . Komabe , Yesu anati : “ Zinthu zosatheka ndi anthu n’zotheka ndi Mulungu . ” Izi zimatithandiza kukhala otsimikiza kuti malonjezo a Yehova amtsogolo adzakwanilitsidwa . Mwacitsanzo , onani kapepala kakuti Kodi Mavuto Adzathadi ? “ Cifunilo ca Atate wanga ndi cakuti , aliyense woona Mwana ndi kukhulupilila mwa iye akhale nao moyo wosatha . ” — Yohane 6 : 40 . ( 2 Akorinto 9 : 15 ) Inde , dipo ndi mphatso yapadela kwambili cakuti sitingakwanitse bwino - bwino kuifotokoza . M’CAKA ca 64 C.E . , Akristu anali kuvutika kwambili ku Roma . Panthawiyo , otsatila a Kristu anali kucitilidwa nkhanza kwambili cifukwa cakuti anali kuwanamizila kuti anayambitsa msokonezo mumzindawo ndiponso kuti anali kudana ndi anthu ena . Ni ufulu wotani umene Yesu analonjeza ? Nanga tingaupeze bwanji ? Iwo akamvetsetsa cifukwa cake , adzakhala ofunitsitsa kukumvelani . 43 : 9 . Cotelo , muyenela kubatizidwa kokha ngati mwafikapo mwakuuzimu , mwamvetsetsa zimene kudzipeleka kwa Mulungu kumatanthauza , ndiponso mwasankha nokha kucita zimenezo . Colinga ca Dziko Lapansi , 6 / 1 Tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi nthawi zonse zoganiza zanga zimakhala pa ndalama ? Kodi inunso mumakonda misonkhano ? ( Mat . 21 : 12 , 13 ) Mwinanso palibe kweni - kweni zimene akanacita kuti athetse umphawi wake . 9 : 1 - 5 , 9 ; 10 : 1 . Kuti tiyankhe funsoli , tiyeni tikambilane za cinthu cina cimene Mulungu watipatsa , cimenenso ni cuma . Nanga mumaŵelenga magazini atsopano ndi mabuku onse atsopano amene amafalitsidwa m’cinenelo canu caka ciliconse ? Nthawi zambili , munthu amapatsidwa ufulu woculuka ngati waonetsa kukhulupilika kwa nthawi yokwanila . Atatuluka m’ndende , anayamba kucita upainiya . Zinthu zina zimene mwana angapemphe zingakhale zosafunikila kwenikweni . ( Pillars of Faith — American Congregations and Their Partners ) Mboni za Yehova zikulalikilabe uthenga umenewu ndipo zimagwilitsila nchito njila zimene Yesu ndi ophunzila ake anaseŵenzetsa . Ise Akhristu tiyenela kudziteteza mwa kusankha zosangalatsa mosamala . Kukhala ndi khalidwe limeneli kumacititsa anthu ena kuti aziticitila nsanje ndi kutida . Koma kodi analimbana nawo bwanji ? Ndi liti pamene ndidzapeza nchito yabwino ? M’Mabaibulo enanso a Cingelezi ndi a zinenelo zina , anacotsamo dzina la Mulungu . 17 : 20 , 21 . 3 : 15 ) Ndiponso , timapemphela ndi kuyembekezela thandizo tikakhala m’mavuto . Nthawi zina tingapeze nkhani zothandiza kapena malemba amene angatilimbikitse kwambili . 30 Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi Posakhalitsa , khamu la anthu aciwawa linafika ndi kuyamba kuponya Paulo miyala . “ Ine ndi mkazi wanga tinali kuganiza kuti Mboni za Yehova zinapezelapo mwai wobwela kunyumba kwathu , cifukwa sitinali kupita ku chalichi . Anali kunena zimenezo cifukwa zinamveka kuti anali kupha ana osalakwa pankhondo . Poyamba mungafunike kudzikakamiza kuti mucite zimene Baibulo limakamba . Mwanjila yozizwitsa , Yesu anapanga vinyo wambili wokwanila anthu onse amene analipo . Ndiponso , Farao sanali kanthu pomuyelekezela ndi Yehova . N’cifukwa ciani tinganene kuti a nkhosa zina amayeletsedwa ndi Mau a Mulungu ? Kumatipatsa mwayi wothandiza ena ndi zinthu zimene tili nazo . M’nkhaniyi , tidzaphunzila mfundo za m’Baibulo zimene zingatithandize kuthetsa mikangano ndi kukhala pa mtendele ndi anthu ena . M’fanizoli , mulinso kapolo amene anali ndi talente imodzi . ( Mac . 13 : 47 - 49 ) Gulu la Mulungu limapeleka malangizo oyenela ogwilila nchito imeneyi . Tsiku lina , iye ananiuza kuti anapatsidwapo uphungu wamphamvu na M’bale Joseph F . ( Ŵelengani Aroma 8 : 15 - 17 . ) N’cifukwa ciani tiyenela kutengela citsanzo ca Yesu ? N’ciani cimagwila mapulaneti monga dziko lapansi ? ( Genesis 2 : 15 ) Mulungu adzaononga “ amene akuononga dziko lapansi . ” — Chivumbulutso 11 : 18 . 45 : 6 , 7 . Tikambilana ciani m’nkhani ino ndi m’nkhani yotsatila ? Kodi zinali zocita kukonzekela ? N’kovuta kuti ena apewe kugwilitsila nchito pelefyumu kapena mafuta ena onunkhilitsa kuti amene amadwala cifukwa ca fungo la zinthu zimenezi asalephele kupezeka pa misonkhano yacikristu . Anthu ena amene timakumana nawo mu ulaliki amakana kumvetsela cifukwa cakuti m’mbuyomo anakumanapo na mavuto ena aakulu . Wodala ndi munthu amene inu mwamusankha ndi kumuyandikizitsa kwa inu . ” Mosazindikila kuti io apangana zotani , Yosefe anafika ndi maganizo akuti zonse zili bwino . “ Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba ” Pamene tiganizila za kukwanilitsidwa kwa ulosi wa m’Baibo wokhudza nthawi yathu ino , sitidzasokonezedwa ndi dziko la Satana . Yehova anandithandiza kuongolela maganizo anga ndi kudziŵa zoyenela kucita . Mulungu anapatsa makolo udindo wosamalila ana , osati ambuye ao kapena anthu ena . ( Ŵelengani Levitiko 10 : 8 - 11 . ) 22 : 37 ; Akol . 3 : 23 ) Pa Pentekosite mu 33 C.E . , otsatila a Yesu anayamba kuphunzitsa anthu a mitundu yonse kukhala ophunzila . N’zoonekelatu kuti sitingafune kukhala na mtima ngati wa Nabala , amene sanayamikile zabwino zimene anacitilidwa . Mtumwi Paulo anauza Akristu kuti : “ Muvule umunthu wakale umene umagwilizana ndi khalidwe lanu lakale , umenenso ukuipitsidwa malinga ndi zilakolako zonyenga za umunthuwo . Conco , tingam’funse kuti : “ Popeza kuti anthu ali ndi maganizo osiyanasiyana ponena za helo , nanga inu muganiza bwanji ? ” Kodi Abulahamu anafunika kukwatilanso mkazi wina ? Kodi Yesu pokamba zimenezo anali kulonjeza munthuyo kuti adzapita kumwamba ? Iye analonjeza kuti anchito onse adzawapatsa malipilo oyenelela , ngakhale amene anagwila nchito kwa ola limodzi . Madzulo , mwini munda wa mpesa uja anaitanitsa anchitowo kuti awapatse malipilo . ndipo Mose anayankha kuti : ‘ Ndodo . ’ ( Miyambo 3 : 12 ) Ndiponso , Yehova ndi “ wacifundo ndi wacisomo , wosakwiya msanga . ” Zili ngati munthu amene anali kupita kutali kudziko lina , amene anasiya nyumba m’manja mwa akapolo ake , aliyense pa nchito yake , ndi kulamula mlonda wa pacipata kuti azikhala maso . Tikaganizila za cilengedwe ndi zonse zili mmenemo , sitikaikila kuti Yehova ali ndi mphamvu zocita ciliconse . Anaona kuti anafunikila kucita zimenezi kuti iye ndi banja lake apitilize kutumikila Yehova . Popeza kuti nchito zina zoyeletsa zimafunika kucitika nthawi zonse pambuyo pa misonkhano , koma zina zimacitika pakapita nthawi , nchito yoyeletsa ifunika kuyang’anilidwa bwino n’colinga cakuti nchito zina zisamanyalanyazidwe . Tingathandize bwanji anthu othaŵa kwawo pa zinthu zofunika kwambili ? 78 : 49 - 51 . Kaya tigwila nchito yokonza Nyumba za Ufumu kapena yomanga likulu lathu ku Warwick , New York , tiyenela kuyamikila mwai wotumikila mwanjila imeneyi . Koma Nowa anadziŵanso kuti zinthu zina sangazikwanitse kucita , koma zina angakwanitse . Palibe moto umene unapha anthu ambili ku United States kuposa moto umenewo . ( Luka 23 : 34 ) Inde , Yesu anakhalabe wofatsa ndi woleza mtima pamene anali kuzunzidwa ndi kukumana ndi mavuto . Iye ni citsanzo cabwino ngako kwa tonsefe . — Ŵelengani 1 Petulo 2 : 21 - 23 . Izi zimatithandiza kupanga zosankha zokondweletsa Mulungu , zimenenso zingatisiye na cikumbumtima coyela . 9 - 11 . ( a ) Kodi nsapato zophiphilitsa zimene Akhristu amavala n’ciani ? Patsala kanthawi kocepa , woipa sadzakhalakonso . ” Miyambo imakhala yosiyana mu akacisi osiyanasiyana a Cishinto . Ndipo ngati timalemekeza kwambili buku lake la Yehova , malangizo ake adzakhala umoyo wathu . — Sal . Timayesetsa kuganizila zimenezo . Ndipo sikuti ndi ufumu wina uliwonse . Kodi tidzatengelapo phunzilo pa zolakwa zao ? Kodi ndimwe mmodzi wa nkhosa zina amene akuthandiza odzozedwa panchito yofunika imeneyi ? ( Akol . 3 : 23 ) Kodi nimapemphela , kuŵelenga Mau a Mulungu , kusonkhana , ndi kulalikila nthawi zonse ? N’ciani cingatithandize kukhala wolimba mtima ? Nthawi zina , nimacita kudzigwila kuti nisangomuyankha na mfundo imodzi yacindunji . Tili ndi maumboni ambili oonetsa kuti Yehova akupitiliza kuthandiza anthu ake masiku ano . Apa lomba n’nali kupeza mayankho pa mafunso anga . ( Mlal . 12 : 1 - 7 ) Ndipo ambili amalephela kucita zimene anali kucita kale , kuphatikizapo ulaliki . Kodi Mkhristu wolapa afunika kucita ciani kuti aonetse kuti amayamikila cifundo ca Mulungu ? Anthu oculuka masiku ano amaganiza kuti kukhala na ufulu weni - weni kumatanthauza kucita ciliconse cimene munthu akufuna , mosasamala kanthu kuti padzakhala zotulukapo zotani . Ngati tiyesetsa kuthetsa mikangano n’colinga cofuna kukhazikitsa mtendele , tidzapeza mapindu oculuka . Kwa Aisiraeli a m’nthawi ya Zekariya , Sinara anali malo oyenelela kukhalako zoipa . 17 Cifukwa Cake ‘ Timapitiliza Kubala Zipatso ’ N’cifukwa ciani Yesu “ anakondwela kwambili mwa mzimu woyela ? Masiku ano , pamene nkhondo ya Mulungu ya Aramagedo ili pafupi , ciŵelengelo ca apainiya ku Britain cawonjezekanso . Anita anakamba kuti : “ Ndinaletsedwa kulambila Yehova m’nyumba muli mwanga . Acicepele angaphunzile zambili pa cikhulupililo ca Davide . 14 , 15 . ( a ) Tingaonetse bwanji cikhulupililo pa umoyo wathu ? Yehova amadziŵa kuti ngati tiŵelenga Mau ake , tidzakhala ‘ olimba mtima ndi kucita zinthu mwamphamvu , ’ m’malo ‘ mocita mantha kapena kuopa . ’ — Yos . Pambuyo pake ndinauzidwa kuti m’matumbawo munali ziwalo za asilikali amene anaphedwa kunkhondo . Komanso , nchito yomasulila Baibo m’zinenelo zokambidwa na ambili inali kuletsedwa . — w17.09 , peji 19 - 21 . 2 : 15 - 17 ; 3 : 15 ) Maganizo aconco angapangitse Mkhristuyo kucita chimo . Izi zimatheka cifukwa ca nsembe ya dipo ya Yesu , imene ndi njila yaikulu imene Mulungu anaonetsela kuti amatikonda . Ndi bwino kudzifunsa mafunso amenewa cifukwa cakuti anthu m’dzikoli amafuna kuti tizitengela zocita zao . Colinga cimene Mfumu ya Nkhondo imeneyi ikumenyela nkhondo sikulanda madela kapena kufuna kupondeleza anthu . Iye anati : “ Kuti kudzela mwa ine , nchito yolalikila icitidwe mokwanila , ndi kuti mitundu yonse ya anthu imve uthengawo . ” M’malomwake , katswiliyo anakamba kuti acinyamata amakonda kucita zinthu zosiyanasiyana , amakhudzika mtima kwambili , ndipo amafunitsitsa kuceza ndi anzao . Thandizo lathu : Cifunilo ca Yehova n’cakuti ‘ onse akumwamba , ndi apadziko lapansi , ’ apinde maondo ao . Pemphelo lingakuthandizeni kupeza “ mtendele wa Mulungu , ” umene ungacepetse nkhawa zanu . — Afilipi 4 : 6 , 7 . 23 Wacicepele , Limbitsa Cikhulupililo Cako Kumbukilaninso kuti ngati munthu afufuza payekha malemba m’Baibulo , kapena kukonzekela zimene adzayankha pa misonkhano , iye adzapindula kwambili kuposa mmene angapindulile ngati mwam’tumila zinthu zimenezi . Coyamba , muyenela kuwauza momveka bwino mfundo za m’Baibo zimene imwe mumatsatila . “ MWANA mbuu make mbuu . ” Ngakhale kuti ophunzilawo anadziŵa kuti kugwila nchitoyo kudzakhala kovuta , io anamvelabe lamulo la Yesu , ndipo analalikila mu Yesusalemu , ku Samariya , ndi kumaiko ena . Kodi unamvelako anthu amene amakamba kuti amakhulupilila cisanduliko cifukwa ni sayansi , osati za Mulungu cifukwa amati ni za cikhulupililo cabe ? 20 : 5 ) Mtumwi Paulo anayesetsa kucita zinthu ndi “ anthu osiyanasiyana ” mowaganizila n’colinga cakuti awalalikile uthenga wabwino . Kodi Yosefe wa ku Arimateya anali ndani ? 1 : 15 ; Sal . Popita ku cikondwelelo ca Pasika ku Yerusalemu , Aisiraeli anali kucita zinthu mogwilizana . Koma cosangalatsa koposa n’cakuti Yehova ndi Yesu Kristu amasamalila anthu a Mulungu . Komabe , nthawi zambili makolo athu anali kukaikila ngati Jairo angaphunzile Baibulo . Ngakhale ndi conco , pali anthu ambili amene amagwila nchito mwamphamvu koma amasangalala ndi nchito yao . Cifukwa ca ici , anacitapo kanthu kuti akwanilitse colinga cawo . Mark Noumair Ndife oyamikila kuti Mulungu ali nafe ndipo amatidalitsa cifukwa ca kuyesayesa kwathu . 19 Tulilani Yehova Nkhawa Zanu Zonse Mzimu umenewu umatithandiza kucita zinthu zambili kuphatikizapo kumvetsetsa Malemba . Funso limeneli linafunsidwa kwa oŵelenga nyuzipepala ya ku Australia yochedwa The Sydney Morning Herald . 89 pelesenti ya anthu amene anapeleka mayankho anakamba kuti cipembedzo cimatigaŵanitsa . Ngakhale zinali conco , Yehu anauzanso Yehosafati kuti : “ Pali zinthu zabwino zimene zapezeka mwa inu . ” — 2 Mbiri 18 : 4 , 5 , 18 - 22 , 33 , 34 ; 19 : 1 - 3 . ( Ŵelengani 1 Timoteyo 6 : 18 , 19 ) Kucita utumiki wanthawi zonse kungakupatseni mwayi wodziŵana ndi atumiki anzanu anthawi zonse , ndipo kungakuthandizeni kukhala Mkhristu wofikapo kuuzimu . N’cifukwa ciani tifunika kucita zinthu mokoma mtima ndi mwacikondi na Akhristu anzathu ? ( Ŵelengani Yohane 5 : 19 . ) Musamacite zinthu zosafunika kweni - kweni , zimene zingakuonongeleni nthawi na mphamvu . Iye anaimilila m’mbali mwa nyanjayo n’kumayang’ana ophunzilawo . Buku lodalilika kwambili la malangizo anzelu limati : “ Odala [ acimwemwe ] ndi anthu osalakwitsa kanthu m’njila zawo . ” Njila imeneyi inandithandiza kusamalila banja langa ndi mabanja ena kwa nthawi yaitali . ” ( Yakobo 4 : 8 ) Ndipo ndimasangalala kwambili ndi ciyembekezo codzaonananso ndi atate anga m’dziko latsopano . — Yohane 5 : 28 , 29 . ANTHU ambili amadziŵa kuti Yesu anali ndi atumwi 12 . Kodi ndimwe wacicepele , kapena mukukalamba ? Kodi tikukhala m’nthawi yotani ? ( Luka 4 : 5 , 6 ) Olo kuti pali cisonkhezelo coipa ca Satana , maboma ambili amayesako kucitila nzika zawo zinthu zabwino . Kuyelekezela Zinthu Kopindulitsa Kwambili ( zikhulupililo na Baibo ) , Na . Kapena cangu canga cayamba kuzilala ? ’ Ena amakonda mabuku a Uthenga Wabwino cifukwa m’Malembawo Yesu anaonetsa makhalidwe okhumbilika a Yehova . Satana amadziŵa zimenezi , ndipo amagwilitsila nchito “ aneneli onyenga ” kuti ‘ awasoceletse . ’ Panapangiwa makonzedwe akuti mipingo iŵili ya zinenelo zosiyana , kapena ya mitundu yosiyana , nthawi zina izisonkhana pamodzi kumapeto kwa wiki . Koma kuti zimenezi zitheke , mbeu inafunikilanso kutumikila pa udindo waunsembe . Conco , sitimanena kuti Akristu odzozedwa ‘ adzakwatulidwa ’ cifukwa cakuti anthu amalimva molakwika liuli . Koma adzatengedwa m’kanthawi kocepa . Zinthu zambili zimafunika thandizo la Yehova kuti tikwanitse kuzicita . Tiyembekezelanso kudzalandila moyo wosatha , wa “ kumwamba kwatsopano ” kapena wa pa “ dziko lapansi latsopano . ” 7 , 8 . Nikamacita mapulakatisi m’bwalo la maseŵela panthawi ya cakudya , sin’nali kumvela njala . M’nkhani ino , tikambilana zocitika zina za m’nthawi ya atumwi zimene zinapangitsa ophunzilawo kulalikila popanda zovuta . Yehova anauza anthu ake kuti : “ Usacite mantha , pakuti ndili nawe . ( Ŵelengani Deuteronomo 26 : 8 . ) Conco , makolo sadziŵa zimene angacite . Hana analonjeza kuti adzapeleka mwana wake Samueli ku cihema kuti azikatumikila monga Mnazili . ( Yobu 14 : 7 - 12 ; 19 : 25 - 27 ) Munthu akafa , sangauke yekha kumanda n’kukhalanso na moyo . ( 2 Sam . 12 : 23 ; Sal . Mulungu wokhulupilika , amene sacita cosalungama . Iye ndi wolungama ndi woongoka . ” — Deuteronomo 32 : 4 . Mpingo winanso mu mzinda wa Izmir unalemba kuti : “ Munthu woseŵenza pa malo okwelela matakisii anafikila mkulu n’kumufunsa kuti : ‘ N’ciani cikucitika ? ’ 24 : 14 ) Mwacitsanzo , mtsikana wina wang’ono ku India anasunga kabokosi , ndipo anayamba kuikamo tundalama twasiliva . Popanda pulojekita yoonetsela filimu kapena cinsalu cacikulu ca pacipupa , Ophunzila Baibulo anali kugwilitsila nchito seŵelo la mau okha limeneli kwaulele kuti afalitse uthenga wa Ufumu m’midzi ndi m’magawo atsopano . Fanizo la Paulo lionetsa kuti anthu onse mumpingo wacikristu ndi ofunika . Satana amafuna kuti tiziganiza kuti ndife osanunkha kanthu . Aperisiya atagonjetsa mzinda wa Babulo , anamasula Ayuda mu ukapolo na kuwalamula kuti akamangenso kacisi wa Yehova ku Yerusalemu . 30 : 23 - 25 . A Daka : Kodi mutanthauzanji ? Nkhani iyi , idzatithandiza kudziŵa mmene tingaseŵenzetsela mfundo ya m’fanizo la Yesu la wamalonda amene anali kusakila ngale . Kampeniyo inathandizadi kuti anthu ambili amvele uthenga wabwino . Amacita zimenezi mwa kutipatsa malangizo opatsa moyo kupitila m’Mau ake . Polalikila uthenga wotonthoza wa Ufumu , n’nali kuona nkhope za anthu zikuwala . ” ( Habakuku 2 : 3 ) Kuti tidziŵe ngati cikhulupililo cathu n’colimba , tifunika kudzifunsa kuti : ‘ Kodi nchito yolalikila ndi yofunika kwambili kwa ine ? Masiku ano , Yehova amapeleka malangizo kwa anthu ake mwa kugwilitsila nchito Baibulo , mzimu woyela , ndi mpingo . ( Mac . Conco iwo anada nkhawa , ndipo anauza Aroni kuti : “ Tipangile mulungu woti atitsogolele , cifukwa sitikudziŵa zimene zacitikila Mose , amene anatitulutsa m’dziko la Iguputo . ” — Eks . Pali zinthu zambili zimene tingacite zoonetsa kuti timakonda Yehova . M’nkhani ino , tidzakambilana njila zosiyana - siyana zimene tingaonetsele kuti timamuyamikila Yehova potipatsa mwayi wapadela umenewu . Akristu onse ayenela kumvela lamulo limeneli mwa kulalikila Uthenga wa Ufumu ndi kupanga ophunzila . A Nicole anati : “ Ndinakwiya kwambili pamene mwana wanga wa mwamuna anamenya mlongo wake . Koma pa zinthu zina , kuphonya m’kamvedwe kungakhudze kwambili umoyo wathu . NYIMBO : 63 , 43 Khalanibe wokhulupilika . 6 : 5 ) Sizikanatheka kuti mngelo akambe mau amenewa . Makolo , kodi mungakhale bwanji bwenzi la ana anu ? Sitifunika kudelela msampha wa ciwelewele kapena kuopsa kwa khalidwe la kunyada . Yesu anatiphunzitsa kuti ‘ tizifuna - funa Ufumu coyamba ’ osati zinthu zakuthupi . Zioneka kuti aliyense wa iwo anali woyamba kubadwa . Koma ndani amene ali anthu ake padziko lapansi masiku ano ? ( Chivumbulutso 11 : 18 ) Kodi anthu akuononga dziko m’njila ziti ? ( Yobu 1 : 9 - 11 ; 2 : 4 , 5 ) Koposa zonse , tifunika kudalila Yehova kuti atipatse mphamvu kuti tipilile . Katatu pa caka , Mboni za Yehova zimacita misonkhano yadela ndi yacigawo , kumene anthu ambili amamvetsela nkhani za m’Baibulo . ( Mat . 26 : 28 ; 27 : 33 ) Mkate ndi vinyo za pa Cikumbutso zimaimila nsembe ya Yesu ya mtengo wapatali imene anapeleka kaamba ka anthu omvela , ndipo timayamikila mphatso yacikondi imeneyi . Conco , n’koyenela kuti aliyense akonzekele mwambo wa Mgonelo wa Ambuye umenewu . Komabe , makolo anzelu amaika malamulo oyenelela na kuphunzitsa ana awo kutsatila malamulowo . Colinga cinali cakuti anthu azicita kuopelatu kuŵelenga Baibo na kukaikila ziphunzitso za chechi . Kodi Cilamulo ca Mose cingatithandize bwanji pankhani ya mavalidwe ndi kudzikonza ? ( Salimo 139 : 14 ; Chivumbulutso 4 : 11 ) Iye watipatsanso mphatso ina imene imatisiyanitsa ndi nyama . 17 : 18 . Ni mfundo yofunika iti yokhudza kulambila koona imene inachulidwa mu ulosi umenewu ? ( Mat . 6 : 24 ) Anthu amene amacita khama kuti akhale ndi zinthu zambili , amakhala ndi umoyo wopanda tanthauzo cifukwa amafuna cabe kukhutilitsa zilakolako zawo zadyela . Kuonjezela apo , umoyo wawo wa kuuzimu umasokonezeka ndipo sakhala okondwela . ( 1 Tim . 6 : 9 , 10 ; Chiv . Koma aliyense wondikana ine pamaso pa anthu , inenso ndidzamukana pamaso pa Atate wanga wakumwamba . ” 3 : 1 - 5 ) M’mau ake anzelu , Yehova anatipatsa zonse zofunikila , kuti tikhale ndi zikwati zacimwemwe ndi zopambana — inde , pamene tili paulendo wathu wopita ku moyo wosatha . — Mat . Kutsatila malangizo . Iye angathe kuvumbula chimo lililonse lobisika pakati pa anthu ake . Ngati tilola anthu ena kutipangila zosankha , ndiye kuti tasankha ‘ kuwatsatila . ’ Ndinakhumudwa kwambili , koma ndinapitiliza kupemphela kwa Mulungu kuti : “ Ndifuna kukudziŵani , ndithandizeni . ” Anthu ambili anali kukwanitsa kuŵelenga zofalitsazo cifukwa Cingelezi cinali codziŵika . 12 : 12 , 13 ) Ise tonse , kuphatikizapo acicepele , tingalimbikitse Akhristu anzathu mwa kukamba mau olimbikitsa . Pamene anali kuphunzila , anapeza kuti zimene zinalembedwa m’mabukuwo zinali na mau komanso ziganizo zosamveka bwino ndi zolakwika . 16 : 1 ; 2 Tim . 3 : 14 , 15 ) Mwacitsanzo , mwamuna wosakhulupilila , angaletse mkazi wacikhristu kucititsa phunzilo la Baibo lokhazikika kwa ana awo aang’ono , kapena kupita nawo ku misonkhano yacikhristu . Mkazi angafunike kulemekeza zosankha za mwamuna wake wosakhulupilila . Pamene tinafika pa nthambi ku Brazil , tinayamba kuphunzila Cipwitikizi . 17 : 10 , 11 ) Nayenso anaphunzila coonadi ndipo anatumikila mokhulupilika monga mkulu mumzinda wa Ottawa , ku Ontario mpaka imfa yake . Tili na ciyembekezo ca moyo wosatha . 13 , 14 . ( a ) N’cifukwa ciani banja lina limene linasamukila m’dziko lina linasankha kusamukila mumpingo wa cinenelo ca m’dzikolo ? Ngakhale kuti m’mabungwe osiyanasiyana mumacitika ziphuphu , zikuoneka kuti vuto la ziphuphu za m’boma lafika poipa kwambili . Kodi mumakakamiza ena kucita zimene inu muona kuti n’zabwino ? 10 : 1 - 4 ) Nanga zikanatheka bwanji kuti macimo akhululukidwe ? ( Afil . 3 : 14 ) Iwo akuyembekezela mwacidwi nthawi pamene adzalamulila pamodzi na Yesu Khristu mu Ufumu wake wakumwamba . Akristu oona sanyalanyaza kuuzako ena zimene amakhulupilila . Knorr ndi mbale Milton G . Phunzilo loyamba kupita patsogolo anali Chris na Mary Kanaiya . 133 : 1 . ( Ŵelengani Aheberi 12 : 2 , 3 . ) Kudzikonda pa mlingo woyenelela kuli cabe bwino , ndipo n’kofunika . Paulo ananena kuti anthu ena amapindula tikawapatsa zosowa zao , koma ifenso timapindula cifukwa Yehova amatidalitsa . — 2 Akorinto 9 : 11 - 14 . Tiyenela kukhala osamala kwambili anthu akayamba kukamba zandale . Davide atamva fanizolo , anakwiya kwambili ndi zimene munthu wolemelayo anacita . Samangouka basi n’kuyamba kuumba , n’kuyembekezela kuti ciwiyaco cidzakhala bwino . Yesu analonjeza otsatila ake kuti : “ Cifunilo ca Atate wanga ndi cakuti , aliyense woona Mwana ndi kukhulupilila mwa iye akhale nawo moyo wosatha . ” ( Yoh . Kodi mungapilile bwanji ngati munthu amene munali kukonda wamwalila ? Laciŵili linali lokhudza mmene Akristu ayenela kukhalila ndi mmene ayenela kucitila zinthu ndi Akristu anzao . 5 : 8 ; Miy . 3 : 21 ) Ciyembekezo cimatithandiza kuikabe maganizo athu pa malonjezo a Mulungu . 41 : 13 ; 1 Yoh . 5 : 19 . Vuto limene Joshua anakumana nalo n’lofala masiku ano . Koma kudziŵa cabe ziwembu za Satana si kokwanila . ‘ Timayenda modzicepetsa ndi Mulungu wathu ’ mwa kuyesetsa kutsatila mfundo za Mulungu mu umoyo wathu ndi kupewa kukhumudwitsa ena . CIFUKWA CAKE TIFUNA KUDZIŴA NYIMBO : 95 , 74 Ni panthawi iti maka - maka pamene nimalephela kupilila ciyeso ? Amakhala opanikizika maganizo kwambili ndipo cimakhala cosavuta kudwala matenda amene angaphatikizepo BP , matenda a mtima , na kumva kuŵaŵa m’thupi monga nyamakazi , na kumva mutu kuŵaŵa * Musacite manyazi kupeleka mapemphelo ocondelela pamodzi ndi a m’banja lanu . Kodi Mulungu ali patali kwambili ndi anthu cakuti sangathe kutiona ? Komabe , pocita zimenezi , amafunika kudziteteza kuti asatengele matendawo . N’tafika pa cisumbu cimeneci kuciyambi kwa caka ca 1949 , akaidi anagaŵidwa ndi kuikidwa m’makampu osiyana - siyana . Ndine wokondwa kuti iwo tsopano amaŵelenga Baibo na kupezeka ku misonkhano yacikhristu ya Mboni za Yehova . Mwakucita zimenezo , Yesu anali kutengela citsanzo ca Yehova cokhala wofunitsitsa kusintha ngati pakufunika kutelo . Zitanthauza kuti tiziyesetsa kudziŵa zimene abale ndi alongo athu akukumana nazo ndi thandizo limene akufunikila . Nanga buku limeneli lingatithandize bwanji kulambila Mulungu m’njila yovomelezeka ? Yehova Mulungu sasinthasintha . Mosakaikila , io anali kuphunzitsa anthu ena kuti akhale aneneli . Iwo anapeza umboni wosonyeza kuti m’zaka za m’ma 600 B.C.E . , patapita zaka 15 kucokela pamene Mulungu analosela za kuonongedwa kwa mzindawu , Ababulo ndi Amedi anauononga ndi kuulanda . N’zoona kuti cimangoco cinachedwa kuti kacisi wa Solomo , osati wa Davide . Mwacitsanzo , timalangizidwa mmene tiyenela kucitila zinthu ndi anthu omwe si amuna kapena akazi anzathu . Timalangizidwanso mmene tingasankhile mabwenzi komanso zosangulutsa . Ndipo cofunika kwambili ndi kukondweletsa Mulungu . ” CITSANZO CABWINO CA PETULO “ Mwana wanga , khala wanzelu ndi kukondweletsa mtima wanga , kuti ndimuyankhe amene akunditonza . ” — Miy . Ndiye cifukwa cake Baibulo limatilangiza kuti : “ Khalanibe oganiza bwino ndipo khalani maso . Anafunikanso kulinganiza tumagulu twaulaliki kuti tuzilalikila kwa maola asanu , na kuika maganizo pa maulendo obwelelako m’madzulo mkati mwa mlungu . Koma patapita nthawi , ambili mwa mafumu amenewo analeka kumvela Mulungu , ndipo anthu ambili amene io anali kulamulila anatsatilanso citsanzo cao coipa . Wolemba mbili yakale dzina lake Jona Lendering anakamba kuti “ maganizo a Plato akuti mzimu wathu unali kukhala m’dziko labwino koma tsopano ukukhala kumalo osayenela , anapangitsa kuti kukhale kosavuta kusanganiza ciphunzitso ca Plato ndi Cikhristu . ” Cimfine ndi zinthu zina zimene siziyendelana ndi matupi athu , zingatifooketse cakuti zingakhale zovuta kugwila nchito za tsiku ndi tsiku . Pa umoyo wake wonse , ndi kamodzi cabe pamene iye anasiya banja lake kupita kukakhala kwina kwa milungu iŵili . Ndipo kwa milungu imeneyo , tsiku lililonse anali kuyewa kwao . Rahabi anali kukhulupilila kuti Yehova adzam’pulumutsa iye ndi banja lake . Mungawalandile mwa kuwapatsa moni mwaubwenzi , kapenanso kuwathandiza kupeza malo okhala . Koma ngakhale kuti anali kuika maganizo ake pa kulalikila , sikuti iye nthawi zonse anali kungoganizila za ulaliki . 17 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi 9 : 37 ; Yoh . 4 : 35 - 38 . Koma Yonatani anali kuwalemekezabe atate ake . Ndipo Baibulo limasonyeza kuti Satana ndiye anayambitsa mavuto amenewa . Sara anali kukonda kuceleza alendo N’zoona kuti kupatsidwa uphungu kapena cilango sikumasangalatsa . Leon Weaver , Jr . Pamene tikukonzekela Mgonelo wa Ambuye , tiyenela kuganizila zimene mtumwi Paulo analembela mpingo wacikristu ku Korinto . Pamene anali kukambilana , maiyo anakamba kuti panali kusiyana kwakukulu pakati pa Ayuda ndi Asamariya pankhani yacipembedzo . Mngeloyo anauza akazi amenewo kuloŵa mkati kuti atsimikizile kuti munalibe munthu . Colinga cimene Yesu anauzila otsatila ake za cizindikilo ca kukhalapo kwake cinali cakuti adzakhale maso . ( Aroma 14 : 8 ) Umaonetsa kuti tinapempha Mulungu kutipatsa cikumbumtima cabwino . ( 1 Pet . Ngakhale titaonetsa mkristu mnzathu kukoma mtima pa mlingo wocepa , iye angasangalale kwambili . ( 1 Yoh . Titayamba upainiya , zinthu zinayamba kuyenda bwino ndipo sizinali zovuta kupeza zinthu zakuthupi . ” — Yes . Mu 1942 , ndinadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa mu umodzi wa mitsinje yathu yokongola . N’ciani cingatithandize kukhalabe ndi mtima woyamikila ? Anafunika kudalila Mulungu wawo , Yehova , ndi kukhala okhulupilika kwa iye . Amakhala na zizindikilo zocepa za matenda ovutika maganizo Felisa : Ang’ono anga atapita kunyumba ya masisitele ku Zaragoza , amai ndi amalume anga , amene anali wansembe , anaganiza zonditumizanso kumeneko . 16 : 35 ) Conco , iwo “ sanasowe kanthu . ” 18 : 18 - 20 ) Kodi si ndise oyamikila kukhala na akulu acikondi amene amayesetsa kuweluza mwacilungamo ? Dec . Panalibe ciliconse capadela copelekela ufulu wotelo kwa Ayuda . Mwa kucita zimenezi , Aroma anali kutsatila mwambo wawo . Anali na mphamvu zopatsa munthu aliyense wa m’dziko lawo ciliconse cimene iwo afuna . ” malinga ndi Aroma 8 : 15 . Yesu anali kukambilana ndi ophunzila ake powaphunzitsa zinthu zambili . ZAKA zoposa 200 zapitazo , anthu sanali kukhulupilila zonse zimene zalembedwa m’manyuzipepala . Kulimbikitsana n’kofunika kwambili , maka - maka masiku ano , cifukwa Satana akulimbana kwambili ndi anthu a Mulungu . — Akol . 4 : 11 ; Chiv . Ife tonse timadalila malamulo odalilika a cilengedwe amene Yehova ndiye anawakhazikitsa . Izi zidzabweletsa madalitso osaneneka kwa anthu amene “ akumuyembekezela ” moleza mtima . — Yes . 30 : 18 . Masiku ano , sitimenya nkhondo yeni - yeni pocilikiza ulamulilo wa Yehova , koma timaucilikiza mwa kugwila nchito yolalikila mwakhama ndi molimba mtima . N’cifukwa ciani simunayankhe mapemphelo anga ? ” Potsilizila , olamulila anapezadi njila yocitila ndi Ophunzila Baibo . Nthawi zonse , tizionetsa kuti timakonda Yehova ndi anzathu . Vesili lanena kuti : “ Pontiyo Pilato anali bwanamkubwa wa Yudeya . Herode anali wolamulila cigawo ca Galileya . ” Iye anamaliza mwa kubweleza langizo lofunika kwambili ili : “ Musamade nkhaŵa za tsiku lotsatila . ” Akapolo amenewo anacitilidwa nkhanza kwambili pogwila nchito m’minda ya nzimbe . Izi zinayambitsa nkhondo yapaciweni - weni imene inatenga zaka 13 . Nkhondoyo inacititsa kuti dziko la Haiti lidziimile payokha mu 1804 . Malinga n’zimene taona , kodi bwenzi labwino limacita ciani ngati pacitika zinthu zina zimene zingawononge ubwenzi wawo ? Koma Paulo anafuula mokweza kuti : “ Usadzivulaze ! ” 11 , 12 . ( a ) Pankhani yopeleka ulemu , n’cifukwa ciani timafunika kusiyanitsa pakati pa olamulila a boma ndi atsogoleli acipembedzo ? Mfundo yakuti pa nthawi ya nkhondo yoyamba ya dziko lonse imeneyi , Akhiristu amenewa sanali kuloŵa mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu ayi . Conco , ngakhale abale ocepawo amene ananyamula mfuti na kuyenda kunkhondo , pankhondo yoyamba ya dziko lonse , anakanilatu kwa mtu wagalu kuwombela mfuti munthu wina . Baibo imachula angelo maulendo oposa 250 . ( Ekisodo 12 : 46 ) Zimenezi zingaoneke zazing’ono . Zimenezi zinandithandiza kugonjetsa vuto limenelo . Mwacionekele , ena anali kudya ndi kumwa kwambili asanapite ku mwambo wa Cikumbutso kapena panthawi ya mwambowo cakuti anali kulephela kukhala maso mwamaganizo ndi mwa kuuzimu . Farao analamula akazi amenewa kuti azipha ana aamuna aciisiraeli akangobadwa . ‘ Mulungu Anakondwela Naye ’ [ Zinenelo 272 ] N’ciani maka - maka cimene cingathandize ofedwa kuthetsa cisoni ? Amacita zimenezi kuti asakaŵelengedwe mlandu wa zotulukapo zake . Angokunamiza cabe ! ’ N’cifukwa ciani simuyenela kupeputsa mafunso a ana anu ? Ndiyeno , mu 537 B.C.E . , Aisiraeli anamasulidwa ku ukapolo pamene kagulu kakang’ono ka Ayuda kanabwelela ku Yerusalemu kukamanganso kacisi ndi kulambilanso Yehova . Musanapange cosankha , mufunika kuganizila mmene cidzakhudzila banja lanu ndi mpingo ( Onani palagilafu 15 ) ( Luka 19 : 38 ) Tsiku lotsatila , Yesu molimba mtima anathamangitsa anthu adyela amene anali kucita malonda mokwela mtengo m’kacisi ndi kubela anthu . — Luka 19 : 45 , 46 . Abale na alongo a m’mipingoyo anafunika kucitila pamodzi ulaliki , kusonkhana pamodzi , ndi kuitanilana ku manyumba kwawo kuti akadye cakudya . Tinapezanso nyumba yokhalamo , kufupi na sukuluyo . INOKI anakhala na moyo kwa zaka zambili . Manja a Mose akatopa , Aroni ndi Hura anali kuwacilikiza . Seŵelo la m’Baibo limeneli linali kukamba za Timoteyo . Seŵeloli linawagwila mtima kwambili cakuti anakhala ofunitsitsa kukatumikila kumene kunali olengeza Ufumu ocepa . Kodi Yosefe anakhumudwa ndi zopanda cilungamo zimenezi ? Mwacitsanzo , banja lingafune kudziŵilatu ngati zidzakhala zoyenela kuti makolo azikhala ndi ana ao , kunyumba yosungila okalamba kapena kuona ngati pali thandizo lina kudela lao . Yesu ali padziko lapansi , kodi anatsatila motani citsanzo ca Atate wake ? Iwo anali oyamba m’banja lathu kuphunzila na Mboni za Yehova . 12 : 38 , 49 ; 22 : 21 ) Popeza kuti anthu anali kucitila tsankho alendo , Yehova anapeleka njila zowathandizila . ( Aheb . Tikapempha mzimu wake woyela , ndipo iye adzatipatsa moolowa manja . Kodi umoyo udzakhala bwanji mu Ufumu umenewo ? Atsogoleli ambili acipembedzo anali kukamba kuti Mkristu ayenela kukhala wokonzeka kufela dziko lake . 11 : 6 . ( 1 Atesalonika 5 : 14 ) “ Kusamalila ana amasiye ndi akazi amasiye m’masautso awo . ” — Yakobo 1 : 27 . Atangobatizika , anayamba kucita maseŵela olimbitsa thupi ku malo ocitila maseŵela . ( Yohane 1 : 34 , 41 ; 4 : 25 , 26 ) Yesu ataphedwa , anaukitsidwa n’kupita kumwamba . Ndipo Yesu analimbikitsika ngako atamvela mau amenewa kaŵili konse — kuciyambi kwa utumiki wake na pamene anali pafupi kuphedwa . 3 : 10 . Kaya tatumikila Yehova kwa zaka zambili , kapena kwa miyezi ing’ono , tonse tingapite patsogolo pomulambila . Iwo amatsatila malamulo , kukwanilitsa malonjezo awo , ndipo nthawi zonse amakamba zoona . Izi zinatithandiza kuika maganizo athu pa cimwemwe cimene tinali kupeza mu utumiki wathu . ( Chivumbulutso 21 : 3 , 4 ) Ndikuyembekezela kudzaonananso ndi atate anga , cifukwa cakuti m’dziko latsopano , ‘ mudzakhala kuuka . ’ — Machitidwe 24 : 15 . N’ciani cidzatithandiza kuwamvetsetsa anthu amene akuzoloŵela dziko lacilendo ? 3 : 1 - 6 . ( Genesis 1 : 2 ) Kenako Mulungu anati : “ Pakhale kuwala . ” Coonadi Cimene Cimatsogolera ku Moyo Wamuyaya ( Agalatiya 6 : 16 ) “ Amuna 10 ” akuimila anthu amene ali ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi kwamuyaya . Mwacitsanzo , m’zaka za m’mbuyomu , Mboni zacikuda ndi zacizungu m’dzikolo sizinali kucitila zinthu pamodzi momasuka cifukwa cosiyana mitundu . Amayi anga anali na zaka 17 pamene n’nabadwa mu 1960 . Uthenga Wabwino wokhudza utumiki wa Yesu umene Yohane analemba , wakhala magwelo a cilimbikitso kwa Akhristu kwa zaka mahandiledi ambili , ndipo mpaka lomba umatilimbikitsa . Kapenanso mukuona kuti mukhoza kucitako mautumiki ena pampingo wanu . Koma palibe m’bale aliyense wa m’Bungwe Lolamulila amene ali na Webusaiti yake kapena amene amaseŵenzetsa njila iliyonse yocezela ya pa intaneti . Zoonadi , dziko lapansi ndi ‘ mphatso yabwino ’ imene Atate wathu wakumwamba anatipatsa . Mosiyana ndi anthu opanda ungwilo , Yesu sangakopeke ndi zoipa . Iye anasonyeza kuti sangakopeke ndi zoipa pamene anakana ciphuphu cacikulu koposa cakuti apatsidwe “ maufumu onse a padziko ndi ulemelelo wao . ” Kodi Akhiristu ofikapo kuuzimu angathandize bwanji acatsopano kupita patsogolo ? Kodi timayesetsa kupatula nthawi yoŵelenga Baibo tsiku na tsiku ? 8 Umboni Woonetsa Kuti Maulosi a M’Baibo ni Azoona Tikamaphunzila zambili za Yehova , m’pamenenso timayamba kumukhulupilila ndi kumukonda kwambili . ( Luka 23 : 50 ) Mosiyana na anzake ambili a m’khotiyo , iye anali munthu woona mtima , wakhalidwe labwino , ndipo anali kuyesetsa kumvela malamulo a Mulungu . Kodi Yesu anali kukhala ndi anthu otani padziko lapansi ? Mzele wobadwila wa Yesu wolembedwa mu Uthenga Wabwino wa Mateyu umaonetsa kuti anali Yakobo winawake , koma Luka anakamba kuti Yosefe anali “ mwana wa Heli . ” Kale , mabuku athu anali kufotokoza kwambili nkhani za m’Baibulo ndi zimene zikuimila . Ndiyeno , mabulosha ndi mabuku ena anamasulilidwa m’Cituvalu . Mwakutelo , Yehova analola Ababulo kulanga anthu ake osamvela . ( a ) Kodi Yehova amafuna kuti tiziwaphunzitsa bwanji ena ? Komanso , mwaona kuti ngakhale pambuyo pophunzila coonadi , Akhristu amapitiliza kupita patsogolo mwauzimu cifukwa ca mphamvu ya Mau a Mulungu . Baibo imaonetsa kuti anthu okonda zinthu zauzimu ali na mwayi . Ngati takhala ndi vuto linalake kwanthawi yaitali kapena kucitidwa nkhanza , tingaone monga kuti Mulungu sayankha mwamsanga . 1 : 1 ; 2 : 17 . Masiku ano , Yehova sangatipemphe kupeleka nsembe ana athu , koma amatipempha kuti tizimvela malamulo ake . 6 : 13 - 18 ) Nanga pangano limeneli lidzagwila nchito kwa utali wotani ? Komanso ndidzalitumizila njala ndipo ndidzapha anthu ndi ziŵeto m’dzikolo . ‘ Amuna atatu awa : Nowa , Danieli ndi Yobu , akanakhala m’dzikolo , io okhao akanapulumutsa miyoyo yao cifukwa cokhala olungama , ’ watelo Yehova , Ambuye Wamkulu Koposa . ” Kodi amuna ayenela kucita zinthu motani ndi akazi ao ? 7 : ​ 21 - 23 ; 25 : ​ 11 , 12 . Ndipo tinawapezadi anthu amene anali ngati nkhosa . Ngakhale kuti nkhaniyi ifotokoza za mkazi amene anasiya banja lake ndi kupita ku dziko lina kukagwila nchito , malangizo ake akhudzanso amuna . Zimenezi zinawasonkhezela kuyamba kukumbukila imfa ya Yesu caka ciliconse . — 1 Akor . “ Usacite Mantha . Dzifunseni kuti : ‘ Kodi ndimakonda kutumila ena mauthenga ? Ngakhale n’conco , Hana sanadandaule cifukwa cosunga lonjezo lake kwa Mulungu . Kodi mukucilimika pa kulimbana kuti mupeze madalitso a Mulungu ? Sindinali kukhulupilila cipembedzo ciliconse . Kusintha kumeneku kunatithandiza kukhala okonzeka kuvomela ciitano cokatumikila pa Beteli ngati angatiitane . ” Tikamatelo , timalimbikitsana ndi kusonyeza cikhulupililo cathu m’malonjezo a Mulungu . Yehova , Atate wathu wacifundo wakumwamba , ndiye gwelo lalikulu la citonthozo . Baibulo limakamba kuti anthu onse a Yehova , kuphatikizapo acinyamata , adzamutumikila “ mofunitsitsa . ” Malemba amachula mkate nthawi 350 , ndipo olemba Baibulo nthawi zambili akamakamba za mkate anali kunena za cakudya . ( Sal . 141 : 5 ) Kunyada kumatanthauza “ kudziona wapamwamba kwambili ” kapena “ kukhala ndi mzimu wodzikuza cifukwa codziona kuti ndife apamwamba kuposa ena . ” Kukambilana zimenezi kudzalimbitsa cikhulupililo cathu mwa iye pamene tiyembekezela moleza mtima kuti atithandize pa mavuto athu . Zinali zopangidwa ndi mkuwa mofanana ndi za Goliyati , ndipo zinaphatikizapo covala ca mamba a citsulo . Nkhani yapoyela yolengezedwa m’nyuzipepala ya The Irish Times , pa May 20 , 1910 Malinga na kafuku - fuku amene anacitika mu 2012 ku United States , mmodzi pa anthu atatu amene anafunsiwa mafunso , anati kukhulupilila zakuthambo “ kumagwilizanako na sayansi , ” ndipo 10 pelesenti anati “ kumagwilizana kwambili na sayansi . ” “ N’nacita cidwi maningi na mahosi anayi a mitundu yosiyana - siyana ndi okwelapo ake . Kodi mungaphunzile ciani pa nkhani ya mkazi wamasiye ? ( Aroma 15 : 4 ) Si buku la nzelu za anthu , koma ndi “ mau a Mulungu . ” — 1 Atesalonika 2 : 13 . Conco , wophunzila Baibo amene amafuna kusunga zinthu zonse zimene Yesu analamula , afunika kudzikana yekha na kudzipeleka kwathunthu kwa Yehova . Abale na alongo amene anaona cocitikaci , anakamba kuti cinsalu cacikulu cimeneco ca mitundu itatu cinatambasuka bwino - bwino , ndipo pakati pake panali cithunzi ca Yesu . ( Genesis 3 : 1 - 5 ) Yesu Kristu anamucha kuti “ woipayo ” ndi “ wolamulila wa dziko . ” Kodi makolo angathandize bwanji ana awo kukhala atumiki a Yehova ocita bwino kuuzimu ? Pa nthawi ina , Yobu anaphunzitsa anzake atatu njila yabwino yolimbikitsila ena . Anacita izi olo kuti pa nthawiyo , iye anali kufunikilanso citonthozo . Imakwanilitsa cosoŵa cathu . Koma Mlengi amachula nyenyezi iliyonse ndi dzina lake . Kodi ni njila zina ziti zimene abale na alongo mu mpingo angalimbikitsile acicepele ? ( 1 Timoteyo 1 : 13 ) Koma Yehova anayesa mtima wa Saulo ndipo sanamuone monga dothi lacabecabe . Cifukwa cokonda Mulungu , ena asiya nchito zapamwamba n’colinga cakuti atumikile Yehova mokwanila . Olo kuti nimasangalala kulalikila anthu ogontha , sinidzaiŵala zimene zinacitika pamene n’nali kulalika pa mseu . N’nalalikila mzimayi amene si wogontha , dzina lake , Chris Spicer . Ngati cilango ciphatikizapo kucotsedwa pa udindo , kodi cimaonetsa bwanji cikondi ca Mulungu ? Iyo inati : “ Kapolo woipa iwe , ine ndakukhululukila ngongole yonse ija utandidandaulila . Anthu amenewo analidi osiyana kwambili ndi Yaeli , amene anacita zinthu zoonetsa kulimba mtima zimene zinalembedwa pa Oweruza 5 : 24 - 27 . 8 : 23 ) Timoteyo ndi Tito ayenela kuti analimbikitsika kwambili atamvela mmene Paulo anali kuwaonela . Kodi dziko limene Abulahamu analandila linali lalikulu bwanji ? Kodi ndingafune kuti ena azindiona mosiyana ndi mmene ndilili ? Kuyambila kale - kale , anthu okonda Mau a Mulungu akhala akuidziŵa mfundo imeneyi . 22 N’cikondi Cotani Cimene Cimabweletsa Cimwemwe Ceni - ceni ? Ndipo pa ndodo ina anafunika kulembapo kuti , “ Ndodo ya Yosefe yoimila Efuraimu komanso anzawo onse a nyumba ya Isiraeli . ” Kodi ayenela kukhala ndi colinga cotani ? N’zosangalalatsa kwambili kuti patapita nthawi , tonse tinayamba kulambila Yehova . Aisiraeli amene anali akapolo anakhulupilila Yehova ndipo iye anawapulumutsa modabwitsa pa Nyanja Yofiila . Ndimalakalaka mabwalo a Yehova ndipo ndafookelatu cifukwa colakalaka mabwalowo . . . Mkristu amene afuna kuloŵa m’banja ayenela kuleza mtima kuti apeze munthu amene adzam’konda ndi mtima wonse . Nili na mnzanga ( ku lamanja ) , pamene tinali kutumikila monga apainiya apadela ku Mistelbach , m’dziko la Austria Masiku otsiliza ciani ? Pambuyo pa makambilanowo , Henri anazindikila kuti njila yokha imene akanathandizila a m’banja lake kubwelela m’coonadi ni kupilila ciyeso cimeneco mokhulupilika . Ngakhale kuti Hezekiya anatumikila Mulungu ndi mtima wathunthu , iye nthawi ina anacita zinthu zokhumudwitsa Yehova . Tonse tinali kudziŵa kuti posacedwa tidzakumana ndi mayeselo aakulu . Nayenso Yobu wa m’nthawi zakale , anali na ciyembekezo cakuti akufa adzauka mtsogolo . Mkwiyo wa ndani ? Iye anati : “ Mau otuluka pakamwa panga . . . sadzabwelela kwa ine popanda kukwanilitsa colinga cake , . . . ndipo adzakwanilitsadi zimene ndinawatumizila . ” Asanakambe izi , iye anati : “ Lekani kudziunjikila cuma padziko lapansi , pamene njenjete ndi dzimbili zimawononga , ndiponso pamene mbala zimathyola ndi kuba . Ponena za Mulungu , wamasalimo analemba kuti : “ Iye amacilitsa anthu osweka mtima , ndipo amamanga zilonda zawo zopweteka . ” NKHANI ZOPHUNZILA Yehova Amatiumba , June ( Aroma 1 : 20 ) Ndipo tikamaŵelenga Baibulo , timaphunzila kuti Iye ndi wacilungamo ndiponso wacikondi . Nkhani zambili zopezeka m’magazini amenewa , zimatiphunzitsa mmene tingatengele makhalidwe a Yehova ndi zimene tingacite polimbana ndi zofooka zathu . Sitingamvetse mmene Abulahamu anavutikila maganizo , kapena kumvetsa nkhawa imene Sara anali nayo . Komanso amuna ofulidwa anali kuyang’anila akazi a mfumu ku nyumba zacifumu . 13 : 15 ) Milomo yathu iyenela kulengeza poyela dzina loyela la Yehova . Conco , ‘ sangalalani mwa Yehova , ndipo adzakupatsani zokhumba za mtima wanu . ’ — Sal . Ndipo ine ndi Bethel tinayambanso upainiya ndipo unacititsa kuti tilandilenso mwayi wina wa utumiki . Anyamata a m’kabungwe kameneka , amalimbikitsidwa kucita zabwino tsiku lililonse . N’cifukwa ciani umanidela nkhawa ? ” Akazi ambili a pabanja amayamikila citsanzo ca Sara . Iye anati , “ Abale anandipatsa malangizo abwino ndi othandiza . ” Popeza n’nali wacicepele , panali kufunika cilolezo ca atate kuti niloledwe kuloŵa m’dzikolo . Baibulo ndiye buku lofunika kwambili kulisinkhasinkha . Kodi kamvedwe kathu pa mafanizo a Yesu kasintha bwanji ? Kodi masiku ano timaonetsa bwanji kuti timacilikiza ulamulilo wa Yehova ? Kodi Ndani Maka - maka Amacititsa Nkhondo ndi Mavuto ? 5 Fotokozani mwa Malemba zimene zinacitika kuyambila mu 1914 mpaka 1919 . Yesu anakambanso kuti : “ Koma mumanyalanyaza zinthu zofunika za m’Cilamulo , monga cilungamo , cifundo ndi kukhulupilika . ” Kodi kamvedwe kathu ka fanizoli kanasintha bwanji mu 1995 ? Patapita nthawi , tinakwatilana ndipo tinayamba kupilila limodzi mavuto amene tinali kukumana nawo . Tingatengele bwanji citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wodzicepetsa ? Onani polemba kuti MABUKU > BAIBULO , kapena mungaunike QR khodi iyi Khalani na cidalilo conse pa lonjezo la Yehova lakuti : “ Usacite mantha , . . . pakuti ine ndine Mulungu wako . ( Aroma 11 : 25 , 26a ) Pambuyo pake , Petulo analemba kuti : “ Kale simunali mtundu , koma tsopano ndinu mtundu wa anthu a Mulungu . ” MMENE BAIBULO LINASINTHILA UMOYO WANGA : Colinga canga cinali cakuti ndidzakhale katswili woponya zibakela ku China . Paulo analemba kuti “ anthu amene amacita zimenezi sadzaloŵa mu ufumu wa Mulungu . ” Iye ananitumila foni na kuniuza kuti : ‘ Kuno ku Myanmar , nthawi zambili timayenda pa basi . N’zoonekelatu kuti wokutonthozani sanali kusoŵa panthawiyo . Kodi mumayesetsa kuona dzanja la Yehova pa umoyo wanu ? Tikambilana mafunso ati m’nkhani ino ? Abigayeli anali mkazi wa Nabala , munthu wolemela amene anali na nkhosa zambili . Nkhosazo anali kuziŵetela m’dela la mapili , kum’mwela kwa Yuda . ( b ) Timabala bwanji mbewu zatsopano za Ufumu ? Ifenso tingalimbikitsidwe mwa kuuzimu ndi mau ouzilidwa a Paulo . Kenako iye anati : ‘ Iponye pansi . ’ Zidziŵeni bwino zida zofufuzila za m’citundu canu , zopulintiwa ngakhale za pa webusaiti . ( Aefeso 5 : 5 ) Ndinali kuganiza kuti kuona cilengedwe codabwitsa ca Mulungu ndi kumene kunali kofunika kwambili . ANTHU ambili masiku ano amakonda kucita zaciwelewele . ( 2 Tim . 3 : 1 - 5 ) M’mbili yonse ya anthu , “ Yehova Ambuye Wamkulu Koposa , ” wathandiza amuna ndi akazi okhulupilika kwa iye , omvela malamulo ake , ndi amene amagonjela ulamulilo wake . — Ŵelengani Salimo 71 : 5 . ( Ŵelengani Salimo 37 : 3 . ) Kudzozedwa ndi mzimu woyela : Yehova amasankha anthu kuti akalamulile ndi Yesu kumwamba mwa kugwilitsila nchito mzimu woyela . Tiyenela kukumbukila kuti Yehova adzacitapo kanthu panthawi yake yoyenelela . Ndinali munthu wosakonda kuŵelenga ndi kuphunzila , conco ndinali kuvutika kwambili kuti ndiike maganizo pa zimene ndinali kuphunzila m’Baibulo . Naonso anthu anapulumutsidwa . Tsopano , pali Mboni zacangu pafupifupi 8 miliyoni . Ndipo izo zimafalitsa mwakhama uthenga wa Kristu m’zinenelo zoposa 600 , ndipo zinenelo zina zikuonjezeka . 6 : 10 ; 1 Tim . 3 : 8 ) Ndipo Akristu ambili cikumbumtima cao cimawaletselatu kumwa vinyo asanacite zinthu zilizonse za kuuzimu . Komabe , malinga ndi maiko , mikhalidwe imasiyanasiyana . Ndipo akacita zimenezo , sadziimba mlandu . Cikondi “ cimayembekezela zinthu zonse ” zolembedwa m’Baibulo ndipo cimatilimbikitsa kuuzako ena zimene timakhulupilila . ( 1 Pet . Anatipatsa luso loganiza pothetsa mavuto , na luso lokonzekela za m’tsogolo . Anayankha kuti : “ Inde nidziŵa bwino - bwino , ” pamene anali kutuma foni anali mu Colorado ku Patterson ku America . Anthu ena amaganiza kuti Mateyu analemba buku lake m’Ciheberi , kenako bukulo linamasulidwanso m’Cigiriki . Yehova Mulungu * ndiye Mlengi wa zinthu zonse ndipo ndi wamphamvuyonse . Cifukwa ca zimenezi , anthu ambili angaganize kuti iye ndiye amacititsa zinthu zonse zimene zicitika padziko kuphatikizapo zoipa . Mahosi amene akudonsa magaletawo ni a mitundu yosiyana - siyana . Tingapewe bwanji khalidwe la alembi na Afarisi na kutengela Yehova ? 12 : 2 ) Panapita zaka zambili , koma Abulahamu ndi mkazi wake , Sara , anali asanakhale ndi mwana . Iwo amafunitsitsa kuphunzila . Koma ena amene poyamba anali olambila mafano anaona kuti kudya nyamayo ni kulambila fano . ( 1 Akor . Analoselanso kuti Koresi anali kudzaphwetsa madzi a mtsinje umene unali kudutsa mumzinda wa Babulo ndi kuti adzapeza kuti zitseko za mzindawo n’zosatseka . Ndani angakane mwayi ngati umenewu ? Wamasalimo anaimba kuti : “ Ofunafuna Yehova sadzasoŵa ciliconse cabwino . ” Conco , panthawi ya ciweluzo , adzaweluzidwa malinga ndi nchito zao pambuyo pa kuukitsidwa , osati zimene anali kucita asanafe . N’cifukwa ciani maganizo akuti anthu angakwanitse kuthetsa mavuto awo angakhale okopa ? ( Aroma 5 : 12 ) Komabe , monga atumiki oona , timacha Yehova kuti “ Atate wathu . ” ( Yoswa 24 : 2 ) Nanga kodi Abulahamu anaphunzilila kuti za Yehova ? Mulungu wasankha Mwana wake , Yesu , kuti adzalamulile anthu onse . Mungamve cimodzimodzi pamene muŵelenga Baibulo kwa nthawi yoyamba . NSANJE IKULA MSINKHU “ Atate wanga akugwilabe nchito mpaka pano . ” — Yohane 5 : 17 . Pitilizani kukhala olimba mwa kuuzimu ndipo khalani acangu pogwila nchito yolalikila ( Onani ndime 15 ) M’caka cimodzi cabe , anthu oposa 100,000 anaphedwa ku Latin America , ndipo anthu pafupifupi 50,000 anaphedwa ku Brazil kokha . 65 : 2 , 3 . “ Kunena za kumwamba , kumwamba ndi kwa Yehova , koma dziko lapansi analipeleka kwa ana a anthu . ” — Salimo 115 : 16 Pa dziko lonse , ciŵelengelo ca anthu amene akulandila coonadi cikuwonjezeleka . Iwo anakhala mabwenzi apamtima . N’cifukwa ciani mumakhulupilila kuti Yehova nthawi zonse amacita zinthu mwacilungamo ? Kodi inunso , simungakonde kukhala ndi umoyo wofanana ndi umenewu ? Ngati izi zakucitikilani , kodi mungacite ciani kuti mukhalenso na cimwemwe ? Kodi munthu wokhulupilika woyamba , Abele , ‘ anaona ’ malonjezo a Yehova ? N’ciani cinam’thandiza kupilila ? ( 2 Samueli 13 : 28 - 33 ) Koma munthu wocenjela coyamba amaganizila za mavuto amene angabwele . Mmene anthu anali kugwilitsila nchito gulaye pomenya nkhondo m’nthawi zakale ( Chivumbulutso 21 : 4 ) Limeneli ndi tsogolo labwino kwambili kwa anthu amene amayamikila cikondi ca Mulungu ! Kodi mungawathandize bwanji odwala na okalamba ? Pamsonkhanowo , Paulo anakamba nkhani mpaka pakati pa usiku . Kodi okwatilana angalimbitse bwanji cikwati cao ? Nthawi zambili , anthu amene amakhala na zolinga zimenezi sazikwanilitsa , ndipo amakhala na nkhawa kwambili komanso amapwetekedwa mtima . Pofuna kutithandiza kuti tizisankha mwanzelu , Yehova anatipatsa cikumbumtima . Pa webusaiti yathu , pali magazini ndi mabuku ena ophunzilila Baibulo . Ndipo zimenezi n’zofala pakati pa acinyamata amene sasamala katundu cifukwa sanakumanepo ndi mavuto . Anawatsimikizilanso mwa kuwauza kuti : “ Atate wanu amadziŵa zimene mukufuna musanapemphe n’komwe . ” N’cifukwa ciani ni yofunika maningi ? Iye anapempha amayi kuti aziwaphunzitsa Baibo . Nthawi zonse , Yesu anali kuganizila zinthu zimene zikanalimbitsa ubwenzi wake na Mulungu . 20 , 21 . N’cifukwa ciani kugwilitsila nchito mafunso n’kofunika ? Mwina kale ena anali kucita ‘ zinthu zimene tsopano amacita nazo manyazi , ’ zimenenso zikanawacititsa kuyenelela imfa . ( 2 Mbiri 17 : 7 - 10 ) Anakafika mpaka ku dela la lamapili la Efuraimu , mu ufumu wakumpoto wa Isiraeli , kuti akalimbikitse anthu ‘ kubwelela kwa Yehova . ’ Wamasalimo anadabwa kwambili atazindikila kuculuka kwa zinthu zabwino zimene Yehova anam’citila . — Ŵelengani Salimo 40 : 5 ; 107 : 43 . Tsiku lina ine ndi Bud tinakumana na m’busa wa cipembedzo ca Church of Christ . Russell . Komabe , zinthu sizinasinthe kweni - kweni . Kodi “ paladaiso ” amene Paulo anaona m’masomphenya n’ciani ? Baibo imafotokoza bwino cimene cinasonkhezela Mulungu kupeleka Mwana wake monga dipo . Imati : “ Mulungu anatisonyeza ife cikondi cake pakuti anatumiza m’dziko Mwana wake wobadwa yekha kuti tipeze moyo kudzela mwa iye . ( Akol . 3 : 10 ) Monga mmene mtengo umabalila zipatso ngati usamalidwa bwino , nayenso munthu amaonetsa makhalidwe amene mzimu woyela umabala ngati alola mzimuwo kum’tsogolela . — Sal . Ayi ndithu . Baibo imati : “ Ciliconse cimene iye anali kucita Yehova anali kucidalitsa . ” — Gen . Mau aulemu adzamanga cikwati canu monga madaka omangila nyumba ( 2 Timoteyo 3 : 2 ) Ngati pakhala vuto la ndalama kapena ngati nchito n’zovuta kupeza , ambili amaona kuti palibe vuto kuba , kunama kapena kucita zinthu mosaona mtima . * Ndi uthenga wofunika uti umene Yehova watituma kukalengeza ? Conco , n’kofunika kulandila uphungu ndi mtima wonse . — Ŵelengani Salimo 141 : 5 . Kodi mwamuna ndi mkazi angaonetse bwanji Khalidwe Lopambana ? Tate wina ku Togo anasimba kuti , “ Kulambila Yehova sikuyenela kukhala kocititsa ulesi . ” ( Luka 2 : 19 , 34 , 35 , 48 , 51 ) M’macaputa aŵili oyambilila a Uthenga Wabwino wa Luka , dzina la Mariya limachulidwa ka 15 , koma la Yosefe limachulidwa katatu cabe . Ndi zitsanzo zabwino ziti zimene tili nazo za anthu amene anayamikila colowa cao cakuuzimu ? Pambuyo potaikilidwa zonse anati : “ N’nali kuona kuti onse acitila pamodzi zinthu koma ine nili nekha . Kodi kulemekeza cikhalidwe ca kumene tikhala kungathandize bwanji kuti tikhale alendo abwino ? Mulungu anadalitsa Nowa ndi banja lake ndipo anawalamula kuti : “ Mubelekane , muculuke , mudzaze dziko lapansi . ” ( Gen . TSAMBA 27 Conco , olo kuti tili m’nthawi zovuta , tingathe kukhala na cimwemwe ceni - ceni ndi cokhalitsa . Kucita zimenezi kunali “ kusaganiza bwino ” cifukwa dzikoli linali la Akatolika . Pamene munthu wina anatiwopseza , n’nafotokozela wapolisi . Maiyo anali kukamba Phili la Gerizimu , limene linali pa mtunda wa makilomita 50 kumpoto kwa Yerusalemu . Mlongo wina amene ali mu utumiki wanthawi zonse , ndipo anasamukila kudziko lina anati : “ Kungolandila ka khadi kosonyeza kuyamikila zimaonetsa kuti ena amakuganizila , ndipo amakondwela ndi utumiki wako . ” Muzikumbukila kuti mufunika kukhala okhulupilika kwa Mulungu . August Krafzig , anapatsidwa nchito yosamalila katundu , ndipo anayamikila kwambili nchito imeneyi . Coyamba , iwo analeka kukhulupilila Yehova ndipo anakana kumvetsela Mau ake . Iye amaona atumiki ake kuti ndi “ zinthu zamtengo wapatali zocokela ku mitundu yonse . ” ( Hag . Kodi Marita anali kukhulupilila ciani ponena za mlongosi wake ? ( Luka 24 : 44 ; Agal . 3 : 24 ) Colinga cake citakwanilitsidwa komanso Mesiya atabwela , Yehova anamuseŵenzetsa pamodzi na ophunzila ake povumbula zambili zokhudza Satana na angelo amene anakhala ku mbali yake . ( 1 Petulo 5 : 7 ) Baibo imatsimikizila kuti Mulungu angakuthandizeni kutsiliza nkhawa zanu . ( 1 Petulo 3 : 18 ; Machitidwe 10 : 40 ) Kodi Yesu anali kuoneka bwanji ataonekela kwa ophunzila ake ? Anapeza citonthozo ceni - ceni kwa Mulungu Wamphamvuyonse . Ine ndi David tinali ndi colinga cakuti tikhale akatswili ochuka ovina . Iye anawauza kuti : “ Kodi Mulungu sindiye amamasulila maloto ? Anthu amafunitsitsa mtendele . M’malomwake , iwo anali kumasuka kucoka m’cipembedzo conama , na kuthandizanso ena kucokamo . Mkwatibwi ameneyu si munthu weni - weni . Koma akuimila gulu lonse la Akristu odzozedwa a 144,000 . Mofanana na zilako - lako zina zacibadwa zimene tili nazo , cilako - lako cofuna kukhala wodziŵika kwa ena cingatisoceletse . ( Agal . 4 : 9 ) Akhristu a m’nthawi ya atumwi amenewo , anali atapita kale patsogolo mwauzimu mpaka kufika pokhala odziŵika kwa Mulungu . Nkhondoyi inasakaza maiko pafupi - fupi 30 . Komabe , ngati zosankhazo sizisemphana ndi malamulo a Mulungu , mkazi wogonjela afunika kutsatila zimenezo . — 1 Pet . Iye potitsogolela amatiuza cabe maganizo ake . 6 : 9 - 13 ) Koposa zonse , “ zopempha zanu zidziŵike kwa Mulungu . ” Ngakhale kuti malangizo a Yesu ndi omveka bwino , machalichi ambili amatangwanika ndi kupemphetsa ndalama kuti aziyendetsela chalichi cao ndi kulipila atsogoleli ao ndiponso anthu ena . Baibulo limanena kuti Satana ndi ziŵanda zake “ akusoceletsa dziko lonse lapansi , ” ndipo akucititsa ‘ masoka padziko lapansi . ’ ( Maliko 4 : 39 ) Pamenepa , Yesu anali kulamula mphepo ndi nyanja kuti zikhale cete ndipo zisayambenso kucita zimenezo . Citsanzo cina ndi dziko la Nepal kumene kuli anthu oposa 29 miliyoni . Ndinadziŵa kuti ndikacoka panyumba , ndidzafunika kupilila ndi anthu amene anali kundiyang’ana . N’ciani cingatithandize kuti tiziona anthu a ku maiko ena monga mmene Yehova amawaonela ? Kwa nthawi ndithu , n’natumikilako pa ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova ku Mexico monga wanchito wodzipeleka . Ndipo timafunikila kwambili thandizo la Mulungu maka - maka ngati tasemphana maganizo na m’bale kapena mlongo wathu mu mpingo . ( Deuteronomo 6 : 1 ) Mose anali atatsogolela anthuwo kwa zaka 40 , ndipo anali kufuna kuti iwo akhale olimba mtima kuti akakwanitse kulimbana ndi mavuto amene angakumane nawo mtsogolo . Tertullian , wolemba mbili wa m’zaka za m’ma 100 C.E . , anakamba kuti anthu ena amene sanali Akhristu anali kukamba kuti : “ Iwo [ Akhristu ] amakondana . . . 13 : 48 ) Conco , tiyenela kukhala ndi maganizo oyenela ndi kuona moyenela anthu amene timapelekela uthenga wabwino wa ufumu . Makolo anga anali kukondana kwambili ngakhale kuti anali ndi zikhulupililo zosiyana . Mumzinda wa Uri , anthu ambili anali kupitana - pitana m’tumiseu , sitima zinali pilingu - pilingu m’madoko , ndipo m’tumashopu munali kupezeka katundu wambili . Pokhala Akhristu , timafunika kudzisamalila ndi kusamalilanso mabanja athu mwakuthupi . ( 2 Maf . 15 : 1 - 5 ) Onani kuti ngakhale kuti ‘ anthu anali kufukizabe ndi kupeleka nsembe yautsi m’malo okwezeka , ’ Azariya “ anapitiliza kucita zolungama pamaso pa Yehova . ” Iye analinganiza magulu a anchito , simbi , mkuwa , siliva , golide mitengo . Mofanana ndi Davide , tifunika kukhulupilila Yehova . Tifunikanso kutumikila iye yekha ndi kumuopa . Ŵelengani Salimo 45 : 4 . Ngati n’conco , ndinu mmodzi mwa anthu oposa 2 biliyoni pa dziko lapansi amene amakamba kuti ndi Akhiristu . Ngakhale tipemphele bwanji , kapena tifufuze bwanji , sitingapeze mayankho otsimikizika pa mafunso a mtundu umenewu . OPEZEKA PA CIKUMBUTSO ( 2014 ) Malemba amatilimbikitsa kuti tifunika kukhala oceleza . Ngakhale anthu amene sadziŵa Mulungu woona , nthawi zambili amacitila ena cifundo . ( Gen . N’tafika zaka 16 , n’nadzipeleka kwa Yehova , ndipo n’nabatizika pa July 24 , 1954 , pa msonkhano wacigawo ku Toronto , m’dziko la Canada . Hosi yacinayi ni yotuŵa , ndipo n’cizindikilo ca matenda ndi zinthu zina zakupha . Wokwelapo wake ni Imfa . Koma n’nadzifunsabe kuti , Ndani analemba maulosiwa ? N’ndani angalosele za kutsogolo molondola conco ? Ngati zinalidi conco , kodi tingaphunzilepo ciani pa nkhaniyi ? Koma pamene ufumu wake unalimba , Rehobowamu anacita zinthu zina zosayenela . Poyamba , Mulungu analenga Mwana wake wobadwa yekha wauzimu amene ndi Yesu . Kodi Inoki anafa bwanji ? Ndipo muyembekezela mwacidwi pamene sikudzakhalanso njala , umphawi , kuvutika , matenda , ndi imfa . ( Sal . 37 : 10 , 11 , 29 ; 67 : 6 ; 72 : 7 , 16 ; Yes . ( b ) Kodi imwe pacanu mwapindula bwanji na zinthu zimenezi ? Iye anakhalako panthawi ya ulamulilo wa Mfumu yoipa Ahazi . Mulungu adzathetsa nkhondo zonse . — Salimo 46 : 8 , 9 . Kwa Sara , mzindawu sunali cabe malo osungilamo katundu , koma unali wokondeka kwambili . Adamu ndi Hava atadya cipatso , anadziika pamalo akuti sangalandilidwe kukhala m’banja la Mulungu . Filipo atalamulidwa na mngelo wa Yehova , anapita kukakumana ndi Mwiitiyopiyayo ndipo anamulalikila “ uthenga wabwino wonena za Yesu . ” Pa Mateyu 25 : 31 - 33 tinaphunzila kuti Yesu ni amene adzaweluza anthu . Tikakumana ndi zinthu zothetsa nzelu , tiyenela kutsatila malangizo ouzilidwa amene Paulo analembela Akristu a ku Filipi . Iye anati : “ Musamade nkhawa ndi kanthu kalikonse , koma pa ciliconse , mwa pemphelo ndi pembedzelo , pamodzi ndi ciyamiko , zopempha zanu zidziŵike kwa Mulungu . ” Ŵelengani Salimo 45 : 16 . Ndiyeno , kuyambila ca m’ma 9 : 00hrs , n’nali kugwila nchito yochisa zovala . N’ciani cingatithandize tikakumana ndi mavuto aconco ? Mau a Mulungu amati : “ Pokhala pake pali mphamvu ndi cimwemwe . ” Ndiyeno , anamuuza kuti io analonjeza kwa Yehova zinthu zimene zidzasinthilatu umoyo wake . Pambuyo pa 1914 , cimfine ca ku Spain cinapha anthu mamiliyoni ambili . Iye anati : “ Yehova ananitumizila alangizi abwino , ndipo n’namvela malangizo amene ananipatsa , olo kuti cinanitengela nthawi kuti nicite zimenezi . ” 20 : 28 ) Kodi mzimu woyela umathandiza bwanji pa kuikidwa kwa akulu ndi atumiki othandiza masiku ano ? 4 : 4 , 7 , 10 ; 12 : 1 - 5 ; Luka 4 : 16 - 21 ) Komanso , anthu amene anamva Yesu akufotokoza Malemba anakhuzidwa mtima kwambili ndi mau ake . Izi ndi zogwilizana ndi zimene Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Munalandila kwaulele , patsani kwaulele . ” — Mateyu 10 : 8 . Iwo ni amphamvu , koma sikuti ni osagonjetseka . MAPINDU AMENE NDAPEZA : Ngakhale kuti poyamba banja lathu silinafune kuti ndiziphunzila ndi Mboni za Yehova , io tsopano amazilemekeza . Ufumu wa Mulungu uli kumwamba ndipo ukulamulila . — Mateyu 10 : 7 ; Luka 10 : 9 . Iye anati : “ Pelekani . . . za Kaisara kwa Kaisara , koma za Mulungu , kwa Mulungu . ” Mtundu wonse wa Aisiraeli — mwina okwana 3 miliyoni — anamasulidwa mu ukapolo ku Iguputo . Mfundo zina zimene zimafotokoza mau Aciheberi ndi Acigiriki zinalembedwa m’mau amunsi m’Baibulo lokonzedwanso n’colinga cakuti tiziliŵelenga ndi kulimvetsa popanda vuto . Kodi Adamu analiona bwanji cenjezo limenelo ? 5 : 18 ) Magulu aŵili amenewa a anthu anali na maganizo osiyana kwambili pankhani yotumikila Mulungu . Pamenepa tingatengepo phunzilo lofunika kwambili . Kodi matalente amaimila ciani ? Mfundo yocititsa cidwi imene asayansi apeza ni yakuti , “ zikuoneka kuti pali mphamvu ina yake m’thupi lathu imene imapangitsa kuti tizithandiza ena . ” Izi ziyenela kuti zinathandiza kuti azimayi amasiye acigiriki amene anakhumudwa akhalenso omasuka . Timakonda Mulungu ndipo timafuna kumumvela ndi kumulola kutiumba cifukwa tidziŵa kuti malamulo ake amatipindulitsa . “ Ana amafunika kuwapatsa malamulo kuti akule bwino . Ciŵelengelo cimeneci cionetsa kuti pafupifupi munthu mmodzi pa atatu aliwonse amakamba kuti ndi otsatila a Khiristu . Masiku ano , pali machechi ambili amene amati ndi Acikhiristu . ( Luka 8 : 19 - 21 ; 18 : 28 - 30 ) N’zolimbikitsa kuona kuti Yesu amafuna kukhala pafupi ndi anthu amene amadzimana zinthu zina kuti am’tsatile . Katswili wina wa Baibulo anati : “ Liu lacigiriki [ lomasulidwa kuti “ cimphepo camphamvu camkuntho ” pa Maliko 4 : 37 ] limanena za cimphepo coopsa kwambili camkuntho . N’cimodzimodzi ndi kapepala kakuti Kodi Baibo Mumaiona Bwanji ? Nsanja ya Mlonda ya Cingelezi ya March 1 , 1961 , inagwilizanitsa zimenezi ndi zimene Satana anacita , pamene anatenga Yesu ndi kupita naye ku phili lalitali kukamuyesa mwa kumuonetsa maufumu onse a padziko lapansi . Kodi pali cifukwa cokhalila ndi ciyembekezo cakuti aja amene adzaukitsidwa adzakwatila kapena kukwatiwa ? 3 : 1 , 2 ) Tiyeni tipewe kucita ciliconse coonetsa kusayamikila kapena kupeputsa mphatso yapadela yocokela kwa Yehova imeneyi . Koma posapita nthawi itali , n’naloŵa usilikali wa mtundu wina . Panthawi ina , Yesu mwini anati : “ Amene waona ine waonanso Atate . ” ( Yoh . Mulungu afuna kuti anthu ambili akapulumuke Aramagedo . Nanga akhala kuti ? Koma kuti malangizowa akuthandizeni , inu mufunika kuonetsa “ makhalidwe amene mzimu woyela umatulutsa . . . cikondi , cimwemwe , mtendele , kuleza mtima , kukoma mtima , ubwino , cikhulupililo , kufatsa ndi kudziletsa . ” ( Agal . Cinthu coyamba cimene cingatithandize kuti tisatenge mbali m’ndale ndi kuona maboma a anthu monga mmene Yehova amawaonela . Cozizwitsa ca makono cimeneci , catheka kokha cifukwa ca mzimu wa Yehova . ” — Ŵelengani 1 Petulo 4 : 1 - 4 . Abulahamu , munthu wakale wacikhulupililo colimba , anamvela Mulungu ndi kucoka mumzinda wolemela wa Uri , n’kukakhala m’mahema n’colinga cakuti akhale pa ubwenzi wolimba na Yehova . ( Aheb . Mwacitsanzo , Akristu oyambilila anali kukonda kukumana pamodzi kuti alambile Yehova ndi kuphunzila za iye . 1 : 7 , 14 ) Isiraeli wauzimu anamasulidwa mu ukapolo wophiphilitsa kwa Babulo Wamkulu mu 1919 . Kuyambila nthawiyo , kulambila koona kwapitabe patsogolo olo kuti anthu a Mulungu akhala akutsutsiwa mosalekeza . ( Chiv . “ Ndiwe Mkazi Wokongola m’Maonekedwe Ako ” ( Sara ) , Na . Conco tifunika kuyamba kucitapo kanthu kuti tiwaonetse cikondi . 28 ‘ Limba Mtima , Ugwile Nchito Mwamphamvu ’ Tingacitenji kuti ‘ tizikumbukila nchito zao zacikhulupililo , ndi nchito zao zacikondi ’ ? — 1 Ates . Kuti muthetse vuto limeneli , muyenela kusinkhasinkha mmene Yehova amaonela khalidwe la tsankho . ( Mat . 7 : 12 ) Ngati titsatila uphungu wa Yesu umenewu , tidzaonetsa kuti tikucita zinthu mogwilizana ndi “ Cilamulo ” ( kuyambila Genesis mpaka Deuteronomo ) ndi “ Zolemba za aneneli ” ( mabuku aulosi a m’Malemba Aciheberi ) . Izi zigwilizana ndi mau a Paulo akuti : “ Yehova amadziŵa anthu ake . ” — 2 Tim . Cimeneco cidzakhala cikwati cosangalatsa kwambili . Mtumwi Yakobo analemba kuti : “ Ngati wina akusowa nzelu , azipempha kwa Mulungu , ndipo adzamupatsa , popeza iye amapeleka mowolowa manja kwa onse ndiponso amapeleka mosatonza . ” Iye anati : “ Pamene tinafika ku Ghana , tinayamba kulalikila m’mudzi wina ung’ono ndipo tinayamba kufunafuna anthu amene sakwanitsa kumvela . Kenako mmodzi wa akuluwo anati , “ Kunena zoona , palibe zimene tacita kwenikweni . ” ( Luka 5 : 3 - 11 ) Ngakhale n’conco , iye anafunika kugonjetsa mtima wodzikonda . Ndi mmene Akhiristu ena anali kuganizila ngakhale panthawi imene atumwi ena anali moyo . N’zotheka anthu kuphunzila ndi kutsatila mfundo za makhalidwe abwino zimenezi monga mmene anacitila Akristu a m’nthawi ya atumwi . Esau anakhalako m’nthawi ya makolo akale , ndipo n’kutheka kuti nthawi zina anali kukhala na mwayi wopelekako nsembe . Mwacitsanzo , kumacititsa munthu kudziimba mlandu , kusagwila nchito mwakhama , kukhala ndi maganizo ofuna kudzipha , kusoŵa mtendele m’banja , ngakhalenso kutha kwa banja . Kodi mavalidwe anu amalemekeza Mulungu amene timaimila ? ( Num . 1 : 50 , 51 ) Ngati Yehova anali kuteteza mwamphamvu conco zipangizo za pa kacisi , kuli bwanji atumiki ake odzipatulila ndi okhulupilika amene wawasankha kukhala anthu ake ? 1 : 15 , 16 ) Imeneyo inali nthawi imene Mose anabadwa . Tiyeni tikambilaneko zitsanzo zocepa . Yosefe anati : “ Ndingacitilenji coipa cacikulu conci n’kucimwila Mulungu ? ” — Gen . 39 : 6 , 9 ; ŵelengani Miyambo 1 : 10 . Makolo amene amaona zinthu moyenela amazindikilanso kuti ana sangacite zinthu monga munthu wamkulu . Ndiyeno , sinkhasinkhani pa zifukwazo ndi Malemba amene akucilikiza mfundozo . M’nthawi za m’Baibulo , kaŵilikaŵili mbuye sanali kukonda kuuza akapolo ake maganizo ake ndi mmene anali kumvelela . Nanga zimene Baibo imaphunzitsa zingakuthandizeni bwanji masiku ano ? ( b ) Kodi muyenela kuwalanga bwanji ana anu ? Nsanja ya Olonda ya March 15 , 1992 , inakamba kuti mofanana ndi mmene Aisiraeli anakhalila akapolo ku Babulo , m’caka ca 1918 atumiki a Yehova anakhala akapolo a Babulo Wamkulu . Kodi adzacondelela atate ake ndi mlongo wake kuti asamulole kupita kudziko lacilendo ? Nkhani yotsatila ifotokoza zimenezi . Ngakhale kuti lemba la Chivumbulutso 19 : 7 likufotokoza kuti “ mkazi wake wadzikongoletsa ” kaamba ka cikwati , mavesi otsatila sakufotokoza za mwambo wa cikwati . James ndi mkazi wake anali banja lacinyamata la zaka za m’ma 30 . Iwo anali ndi khalidwe lofanana ndi la Smita . Ufumu wa Mulungu ndi boma lenileni limene likulamulila kucokela kumwamba 8 : 8 ) Ngati nkhani yanu ili na autilaini yokonzewa ndi gulu la Mulungu , muyenela kuiŵelenga mosamala pamodzi na malemba ake . Ndimayesetsa kupeza nthawi yoyenela yakuti tiŵelengele pamodzi lemba lina lake kuti ndimuthandize ‘ kutsegula maso ake ndi kuona zinthu zodabwitsa ’ zopezeka m’mau a Mulungu . ’ ( Sal . Pamene Yesu anali ndi ophunzila ake 11 okhulupilika , iye anayambitsa mwambo wa cakudya capadela . Ophunzila ake anafunikila kucita mwambo umenewo caka ndi caka pokumbukila imfa yake . Kodi anacita mantha ? Ena atawapima DNA ndi kupeza umboni wakuti ni osalakwa , anawamasula , koma pambuyo pakuti akhala kale m’ndende zaka zambili . Sindingaleke kukhala Mboni ya Yehova . ” Kungocokela ali mwana , Timoteyo anali kuona mwamuna wolemala ameneyu nthawi zambili m’miseu ya ku Lusitara . 2 : 5 ) Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Mwa cikhulupililo cimeneco , [ Nowa ] anatsutsa dziko . ” KODI Mulungu ali na gulu lake ? Ndipo mtumwi Paulo , amene anakhalako m’zaka 100 zoyambilila , anacenjeza Akhristu za amuna amene anali kudzakamba “ mau ouzilidwa omwe ndi osoceletsa , ” ndi ‘ kuletsa anthu kukwatila . ’ — 1 Timoteyo 4 : 1 - 3 . Koma sadziŵa kuti pakati pa ophunzila ake panalinso akazi ena amene anali kugwilizana naye kwambili . AKULU amene akwanitsapo kuthandiza ena mumpingo anapeleka malangizo awa : NYIMBO : 121 , 75 CINANSO CIMENE MUNGACITE : Muzipatsa ana anu nchito za pakhomo kuti aphunzile kutumikila ena . Udindo wanji ? Koma ise timafuna kukhala odziŵika kwa Mulungu , monga mmene Paulo anakambila , pamene anati : “ Tsopano pamene mwadziŵa Mulungu , kapena tinene kuti tsopano pamene mwadziŵidwa ndi Mulungu , mukubwelelanso bwanji ku mfundo zacibwanabwana , zomwe ndi zosathandiza ndiponso zopanda pake , n’kumafuna kukhalanso akapolo ake ? ” ( Agal . 4 : 9 ) Ndithudi ! Anapitiliza kudziphunzitsa na kudalila mzimu wa Yehova . 4 Kusakila Mphatso Yabwino Koposa Baibulo limakamba kuti anthu ena anali mabwenzi a Mulungu . Tinayesetsa kusamalila nkhaniyo nthawi yomweyo . Mouzilidwa , io analemba mau ocokela kwa Yehova ndi mbili yokhudza ubwenzi wa pakati pa Mulungu ndi anthu ake . Ndiyeno , ipempheleleni nkhaniyo ndi kuona zimene mungacite kuti muwongolele . N’zacisoni kuti makolo ena pambuyo pobwelela kunyumba , amakhumudwa akaona kuti ana ao sawaonetsa cidwi . Iwo anganene kuti , “ N’cifukwa ciani simuyamikila zonse zimene ndimakucitilani ? ” N’kusiyana kwabwanji kumene kulipo pakati pa Bungwe Lolamulila ndi atsogoleli a Machechi Acikhiristu ? KUCIYAMBI kwa caka ca 31 C.E . , Yesu Kristu ali paphili lina limene lili pafupi ndi mzinda wa Kaperenao , anaphunzitsa otsatila ake kupemphela kuti : “ Ufumu wanu ubwele . ” ( Mat . Ulosiwo unakambanso kuti anthu amene amalambila Mulungu m’masiku ano otsiliza adzagwilizana ndi kukhala mtundu umodzi . Iwo anali anthu angwilo ndipo anali kukhala m’paladaiso . Na ise tingakhale na cidalilo conse kuti malonjezo onse a Yehova Mulungu adzakwanilitsidwa , ngakhale mbali iliyonse yaing’ono . Ha ! 11 : 12 , 13 ; Yer . Ciukililo cake cinali umboni wakuti iye analidi Mwana wa Mulungu . Cifukwa ophunzila ake anadziŵa kuti iye ali moyo , io sanakhalenso ndi cisoni kapena kucita mantha . Oweruza Yefita asanapite kukamenyana ndi Aamoni , analumbila kwa Yehova kuti ngati adzamuthandiza kupambana nkhondoyo , ndiye kuti munthu woyamba kutuluka m’nyumba yake kudzamucingamila pocoka ku nkhondo , adzamupeleka kwa Yehova kuti azikam’tumikila ku cihema . 4 : 22 , 23 . DZINA : Linacokela ku liu la Cigiriki lakuti bi·bliʹa , limene limatanthauza “ tumabuku ” Pamene mukupanga zosankha , kodi mumangosankha zimene muona kuti n’zoyenela ? Lelolino , m’gulu la Yehova mufunika anthu ambili odzipeleka kuposa kale lonse . Ndipo timalimbikila kutsatila malangizo amenewo kulikonse kumene tili , kunyumba , mumpingo , kunchito , kapena kusukulu . ( Miy . 7 : 22 ) Zikanakhala zosavuta kuti iye akhale ndi cuma , ulamulilo ndi udindo , zinthu zimene Aiguputo ena sakanakhala nazo . ( a ) Ndi mfundo ziti zimene a m’Komiti Yomasulila Baibulo la Dziko Latsopano anatsatila pogwila nchito yao ? M’malo mofotokoza cabe zocitika za m’Baibulo ndi zimene zimaimila , zofalitsa zathu masiku ano zimafotokoza mmene nkhani ina ya m’Baibulo imagwilizanilana ndi inzake . Cotelo , tiyeni tiyandikile kwambili Yehova mwa kusinkhasinkha phindu la dipo ndi kuphunzila mwakhama Mau ake , Baibulo . — Ŵelengani Deuteronomo 13 : 4 . “ N’nali kuona kuti Baibo si yosangalatsa kuŵelenga . ” — Queennie “ ANAPELEKA MWANA WAKE WOBADWA YEKHA ” Anthu onse amadwala , amakalamba ndi kufa . 3 : 11 ) N’cifukwa ciani pali mafunso ambili conco opanda mayankho ? N’ciani cinathandiza m’bale wina kukhulupilila kuti ali ndi coonadi ? “ Mau a Mulungu ndi amoyo ” Nanga mungaonetse bwanji kuti ndinu olimba mtima ? ( Yes . 5 : 20 ) Cifukwa timafuna kukondweletsa Mulungu , timayesetsa kukhala oyela kuthupi , m’makhalidwe , na kuuzimu . ( 1 Akor . Kodi mkazi anagonjetsa bwanji m’silikali wodziŵa kumenya nkhondo ameneyu ? N’nali kuganiza kuti ni mnzanga wa pamtima ! ’ Fotokozani . N’zomvetsa cisoni kuti Adamu ndi Hava sanafune kuti Yehova aziwalamulila . ( b ) Kodi mfundo zimene takambilana zakucitsani kumva bwanji ponena za Yehova ? Zimenezi zinaonetselatu kuti Jairo anali atapeleka kale moyo wake kwa Yehova . Pulogalamu ya JW Language ingakuthandizeni kucita zimenezi . Mosiyana ndi zimenezi , Yesu Khristu anachula njila yosavuta yopezela ufulu weni - weni . Monga mmene Yehova angakuthandizileni kuphunzitsa ana anu akali aang’ono , adzakuthandizaninso kuwaphunzitsa ngakhale atakhala acinyamata . Kodi zinthu zidzakhala bwanji m’tsogolo ? Komabe , kukumbukila Bungwe Lolamulila sikutanthauza cabe kulipemphelela . Kumaphatikizapo kugwilizana ndi citsogozo cake . Ngakhale kuti anali na udindo wapamwamba , cuma , na ulamulilo waukulu , Nehemiya sanadzidalile yekha kapena kudalila maluso ake . Pa zocitika zonsezi , n’nadziŵa kuti mzimu woyela unali kunithandiza , ndi kuti Yehova ananigwila dzanja na kunilimbitsa . — Yes . Popeza kuti Akristu amenewa sangathe kucita utumiki wanthawi zonse , io amasangalala kuthandiza ana a makolowo kuti apitilize ndi utumiki wanthawi zonse . 16 : 11 - 15 ) Mofananamo , Yesu analoŵa kumwamba kwenikweni ndi mtengo wa magazi ake ndi kuwapeleka kwa Yehova . Ganizilani cabe mmene Sara anayang’anitsitsila mwamuna wake ndi maso ake okongola , na kum’funsa mtima uli m’mwamba kuti : “ Wakuuzani ciani ? Mendo ndi imene inakhala monga manja anga . Onjezelani ciŵelengelo ca magazini amene mumagaŵila . Makolo ena amalephela kulangiza ana awo cifukwa coopa kuwakhumudwitsa . N’cifukwa ciani maboma a anthu sangakwanitse kutsiliza mavuto aakulu amene ise anthu timakumana nawo ? Mwacitsanzo : Ngakhale kuti wophika cakudya amalaŵa pophika , iye sangadalile cabe cakudya colaŵa kuti akhale na moyo . Wacicepele akacita zinthu ngati zimenezi , musalephele kumuyamikila mocokela pansi pa mtima . Kodi Petulo anaonetsa bwanji kuti tingagonjetse mtima wodzikonda ? Komabe , kutumikila ku maiko ena kulinso ndi mavuto ake . Anathandizanso Yobu kuzindikila kuti pali nkhani zina zofunika kwambili zimene anafunika kuziganizila kuposa mavuto ake . Ndinayesetsa kucita zimene ndinali kuphunzitsa , kukhala wodekha , ndi kuwayamikila mocokela pansi pamtima . ” Iye anandisonyeza buku lakuti Coonadi Cimene Cimatsogolera ku Moyo Wamuyaya ndi kundifunsa kuti , “ Kodi mungalikonde buku ili ? ” Njila imodzi imene tingadziyesele ndi mwa kudzifunsa mafunso monga akuti : ‘ Kodi ndimapemphela nthawi zonse ? Palibe munthu amene anatailapo zambili potipatsa mphatso kuposa zimene Yehova Mulungu anatailapo . Komabe , tifunika kukhala osamala . Analinso “ mlaliki wa cilungamo ” ndi wolimba mtima . Anali kulalikila kwa ena za cikhulupililo cake mwa Yehova . ( 2 Pet . “ N’NDANI amakutsogolelani ? ” Pambuyo pooloka mtsinje wa Firate , mwacionekele pa Nisani 14 , 1943 B.C.E . , iwo analoŵela ca kum’mwela kuyenda kudziko limene Yehova anawalonjeza . N’cifukwa ciani n’kofunika kumvetsetsa ndiponso kumvela lamulo la Yehova lokhudza magazi ? Ndipo mukadziyelekezela na mmene iwo amaimbila , mumaona kuti mau anu si abwino kweni - kweni cakuti simungakwanitse kuimba bwino . ( Yer . 30 : 11 ) Kudziŵa mfundo imeneyi kumatithandiza kukhulupilila kuti Yehova anacita zinthu mwacilungamo ndi Azariya ngakhale kuti sitikudziŵa cifukwa cake anacita zimenezo . Kodi panthawi ina munaona kuti simungacite zambili cifukwa ca mmene zinthu zilili pa umoyo wanu ? Ndithudi , kumeneku kunali kusintha kwakukulu kwa ophunzila acangu aciyuda ! — Mac 1 : 8 . Malinga n’zimene Yesu anakambilatu , cinacitika n’ciani mumpingo wacikristu woyamba ? Cimene ciyenela kusonkhezela munthu kuti abatizike ni kuyamikila kwake coonadi na mtima wonse , na kufunitsitsa kwake kusenza udindo wokhala wophunzila wa Khristu . — 2 Akor . Zosangulutsa zimatitsitsimula ndi kutithandiza kupezanso mphamvu . Ndiyeno Yehova anamukantha ndi khate . — 2 Mbiri 26 : 3 - 5 , 16 - 20 . Coyambilila , akuyesa - yesa kuti ayenelele kukhala mtumiki wothandiza . N’cifukwa ciani tingakhale otsimikiza kuti Yehova adzakwanilitsa colinga cake cokhudza mtundu wa anthu ? Pofika m’caka ca 1923 , ndalama ya ku Germany inathelatu mphamvu . Kaya ndise acikulile kapena acicepele , tonse tingacite bwino kudzifunsa mafunso awa : ‘ Kodi pali zilizonse zimene zasintha mu moyo wanga zoonetsa kuti nayamba kukhala munthu wauzimu ? Cinanso , tifunika kulandila moyamikila thandizo locokela kwa ena . — w18.02 , peji 26 . ( Nyimbo 1 : 6 ; 2 : 10 - 15 ) Ngati muli pa cisumbali , n’ciani cimene muyenela kupewa kuti musacite ciwelewele ? Anthu aconco amalakalaka kuti akayanjanenso ndi anzao a m’cikwati akadzaukitsidwa m’dziko latsopano . Simone anadzionela yekha kuti Mau a Mulungu ni amphamvu . 13 Tengelani Cilungamo ca Yehova na Cifundo Cake Dokowe Zingatheke bwanji zimenezi ? Imeneyi inali Baibo yoyamba ya Cigiriki yokhala na mabuku onse a malemba amene ena amati Cipangano Cakale . Kodi tingalemekeze bwanji cikumbumtima ca Akristu anzathu ? Gagik anati : “ Ndalama zimene n’nali kupeza zinali zocepa kwambili , ndipo cinali covuta kusamalila banja langa . Cifukwa ca cikhulupililo cathu , “ sitikubwelela m’mbuyo . Koma ngakhale munthu wathu wakunja akutha , ndithudi munthu wathu wamkati akukhalitsidwanso watsopano tsiku ndi tsiku . ” ( 2 Akor . Ndinacotsanso mafano onse a cipembedzo amene ndinali nao . Pa tsiku lothela kukhala ku Yerusalemu , Yesu anakagona mumzinda wapafupi wa Betaniya . ( Mateyu 21 : 17 ) CAKA COBADWA : 1951 Kodi inunso munamvapo ngati mmene Yosefe anamvelela ? Komanso , mtendele ni wofunika ngako m’banja . Nsapato zimene asilikali aciroma anali kuvala zinali zopita nazo ku nkhondo . Dzina la Mulungu linalembedwa m’zilembo zinai za Ciheberi zochedwa Tetragalamatoni . Tonse tili na ufulu wosankha anthu oceza nawo , mavalidwe , modzikonzela , ndi zosangalatsa . Ndinaphunzila zinthu zambili zokhudza Yehova cifukwa cotumikila m’maiko osiyanasiyana Anthu amenewa ni adyela , ndipo amangofuna kukhutilitsa zokhumba zawo . Sindikanatha kuwaŵelengela nkhani za m’Baibulo , kupemphela nao , kuwakumbatila ndi kuseŵela nao . ” Mwa ici , nthawi zina pangabuke mavuto . Zimenezo zikacitika , tinaphunzitsidwa kutsatila malangizo a Yesu akuti : ‘ Yanjana ndi m’bale wako . ’ M’malo mwake , okwatilana amalimbitsa cikwati cao ngati amathetsa mikangano mwamsanga ndi kupewa kukulitsa nkhani . Ngakhale n’telo , Baraki anavomela kupita kunkhondo , koma anafuna kupitila limodzi ndi Debora . — Oweruza 4 : 6 - 8 ; 5 : 6 - 8 . Asa anali mfumu yacitatu yaciyuda kucokela pamene ufumu wa Yuda unapatukana ndi ufumu wakumpoto wa Isiraeli wa mafuko 10 . Davide anaimbanso kuti : “ Nchito zanu zonse zidzakutamandani , inu Yehova , Ndipo okhulupilika anu adzakutamandani . Iye anaiwala kuti Yehova akumuona . ( Gen . 23 : 2 ) M’kupita kwa nthawi , cisoni cimayamba kucepa . — wp16.3 , peji 4 . Odwala akhozabe kumvela pang’ono , olo kuti akuoneka kuti agona . Izi zikutanthauza mamiliyoni mahandiledi ambili , ngakhalenso mabiliyoni , a zolengedwa zauzimu ! M’nkhani yotsatila , tidzaona mmene Mulungu anacitila zimenezi . Pamene n’nali mwana , atate ndiwo anali kunisamalila ngati amayi apita kumisonkhano ndi muulaliki kumapeto kwa wiki . N’cifukwa ciani tifunika kuyesetsa kukhala odziletsa ? Zimene okhulupilila zakuthambo na olosela zakutsogolo amakamba , zimaonetsa kuti tsogolo lathu linakonzedwelatu . Pamene Lefèvre anali kufufuza kuti amvetsetse matanthauzo a zolemba zakale , anayambanso kuphunzila mosamala kwambili Baibo ya Akatolika , ya m’Cilatini yochedwa Vulgate . Kodi nthawi zina Paulo anali kuwagwilitsila nchito motani mau akuti “ wofooka ” ndi “ amphamvu ” ? Koma iye sanafune kuti zimenezo zimusokoneze na kumulepheletsa kuika maganizo ake pa nkhani yofunika maningi ya Ufumu wa Mulungu , umene udzathetsa mavuto onse . Tinayankha kuti , “ Nanga bwanji ngati asilikali a boma atigwila ? Apainiya aŵili , Stuart Keltie ndi William Torrington , anaonetsa khama limenelo . Tinakhala ndi zotsatilapo zabwino cifukwa ca khama lathu loika zinthu za kuuzimu pamalo oyamba . Posacedwa Muzilemekeza Amene Afunika Kulandila Ulemu , Mar . Pokhala mu “ masiku otsiliza , ” tili m’nthawi yovuta kucita nayo . Mulungu wacoka n’kukusiyilani nyumba yanuyi . ” Ndipo amationetsa njila yabwino imene tingakhalile paumoyo wathu . “ Ngati ana athu ajaila kugwila nchito za pakhomo akali pa nyumba pathu , sadzavutika akadzayamba kudzikhalila . Kodi tingakulitse bwanji khalidwe la cifundo olo kuti nthawi zina zimakhala zovuta kutelo ? Muyenela kutumiza ndalamazo limodzi ndi kalata yonena kuti mwangobweleketsa ndalamazo . Conco , nthawi zonse Yehova akatithandiza , timakhala na “ mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse . ” 4 : 15 , 16 . Ophunzilawo anali kukonda Yesu ndi uthenga wabwino . ( 1 Ates . 5 : 11 ) Ngati Yehova wakuthandizani kuti mukwanilitse utumiki wanu , cikhulupililo canu cidzalimba . Zimenezi zidzakuthandizani kuona utumiki wanu kukhala wofunika kwambili kuposa ciliconse cimene dzikoli lingapeleke . M’Baibo muli maganizo a Mulungu , conco tifunika thandizo lake kuti timvetsetse zimene tiŵelenga . Nthawi zonse iye amafufuza Malemba kuti apeze coonadi cozama cifukwa amadziŵa kuti “ cakudya cotafuna ndi ca anthu okhwima mwauzimu . ” Kenako Yosefe anafotokoza kuti anacita kumuba kwao , ndiponso kuti anamuika m’ndende popanda colakwa ciliconse . — Genesis 40 : 9 - 15 . Nanga bwanji za magaleta ? ( 1 Mafumu 18 : 39 ) Ataona zimenezi , anthuwo anavomeleza kuti anaona mphamvu za Mulungu . Kumbukilani citsanzo cija ca munthu amene ali pa sitesheni . Yesu anauza ophunzila ake mwacindunji kuti azicita mwambo umenewu ndipo anawaonetsa mmene ayenela kucitila . MASIKU ano , anthu a Yehova padziko lapansi amam’lambila m’njila imene imam’sangalatsa . M’nthawi zakale , Aisiraeli anali mtundu wosankhidwa wa Mulungu , koma io anakhala ampatuko . ( 1 Yohane 4 : 8 ; Salimo 37 : 29 ) Kodi inu mungacite ciani kuti mukapulumuke cisautso cimeneci ndi kulandila madalitso oculuka ? Komanso , Yesu anakambilatu zocitika za m’tsogolo , kuphatikizapo zocitika zimene zidzakhala cizindikilo coonetsa kuti mapeto a dzikoli ali pafupi . Komabe , abale anali kudziŵa bwino kuti otsatila a Yesu ayenela kucitila umboni za iye “ mpaka kumalekezelo a dziko lapansi , ” kuphatikizapo kumadela akutali kwambili m’dziko la Australia . ( Mac . Koma boma lililonse limanena kuti ulamulilo wao ndiye wabwino . Izi zapangitsa magaŵano pakati pa anthu . Yehova adzacititsa kuti pakhale ofalitsa ena kuti agwile nchitoyo . ” M’kupita kwa nthawi , luso la m’bale , mmene amacitila zinthu , ndi mmene amasamalilila maudindo ake zimadziŵika pang’onopang’ono . Anacita zimenezi kuti m’dzina la Yesu , onse akumwamba , apadziko lapansi , ndi apansi pa nthaka apinde mawondo ao . Muzipempha mzimu woyela , umene ni wamphamvu kwambili m’cilengedwe conse . Ngati musunga cakukhosi , mungaononge thanzi lanu komanso cikwati canu . Kuti mwana wa Yefita akwanilitse lonjezo la atate ake , anafunika kutumikila Yehova nthawi zonse pa cihema . Popeza kuti ‘ nchito zake zonse ndi zangwilo , ’ Mulungu amadziŵa bwino nthawi yoonetsa mphamvu zake zodziŵilatu zamtsogolo malinga ndi colinga cake . ( Salimo 145 : 18 ) Conco , nthawi zonse tikamapemphela , ubwenzi wathu ndi Mulungu umalimba kwambili . 11 : 11 , 12 ) N’ciani cinamuthandiza kukhala ndi ciyembekezo cotelo ? Izi zinalimbitsa ngako cikhulupililo canga . Ndipo tizikumbukila kuti tingathandize kukweza ucifumu wa Mulungu mwa kukhalabe okhulupilika ngati Yobu tikakumana ndi mavuto aakulu . Yehova analenga Yesu asanalenge cina ciliconse . 7 : 12 ) Koma kodi munthu angakhaledi wacimwemwe ngati ali cabe na ndalama zocepa zomuthandiza kugula zinthu zofunikila mu umoyo ? Ndipo mwacionekele , Paulo anagwila mau a pa lemba la Numeri 16 : 5 . Kukhala ndi cikhulupililo ceniceni kumatithandiza kulimbana ndi nkhawa . Sikuti anthu amenewa angotopa ndi moyo wa padziko lapansi . Nkhondo imene inatsatilapo ikuchulidwa kaŵili m’Baibulo , ikufotokozedwa m’caputala 4 ndi m’nyimbo ya Debora ndi Baraki m’caputala 5 ca buku la Oweluza . Zina mwa izo ni izi : Mulungu amaona moyo kukhala wopatulika . Iye anagona ndi mkazi wa Uriya , kenako anauza Yowabu kuti aonesetse kuti Uriya waphedwa ku nkhondo . ( Onani cithunzi pamwamba . ) ( b ) N’cifukwa ciani Petulo anayamba kumila ? Iye amasangalala ndi zinthu zimene analenga , ndipo amafuna kuti nafenso tizisangalala nazo . — Mac . 14 : 16 , 17 . Mwa ici , Eduard Varter anapatsa Nikolai malangizo olimbikitsa akuti : “ Ngati akulu - akulu a boma akufunsa kumene timatenga zofalitsa zathu , mosapita mbali uziŵayankha kuti timazitenga ku likulu lathu ku Brooklyn . Mwamantha , n’nakweza m’mwamba kansalu kawaiti kam’manja . Abale oimilako bungwe lolamulila anatumizidwa kuti akapeleke kalatayo ku mipingo . Panthawi zovuta zimenezi , tingafunikile kusankha kulandila tuzigawo twa magazi ndi njila zacipatala zogwilitsila nchito magazi . Timakhala ndi cimwemwe coculuka cifukwa cotumikila Yehova . Iye anasiya anthu ake akuphedwa m’matope , ndipo anazemba asilikali aciisiraeli n’kuthaŵila kouma kwa anthu apafupi amene anali kugwilizana nao . Mofanana ndi m’bale Sergio na mlongo Olinda , abale na alongo ambili okhulupilika pa dziko lonse lapansi akhala akulalikila kwa zaka zambili m’magawo a anthu opanda cidwi . 5 : 6 . Ndithudi , ngati musinkha - sinkha mozama zimene mumaŵelenga m’Mau a Yehova amtengo wapatali , mudzayamba kukondwela pophunzila . — 1 Tim . Nanga anthu oona mtima angawadziŵe bwanji alambili oona a Mulungu ? Ngakhale n’conco , m’kupita kwa zaka , mau ambili m’Baibo ya King James Version anakhala acikale . Panthawiyo , panalibe nyumba yakuti ticite lendi . Kutamanda “ Ndidzatamanda Yehova nthawi zonse . Ndidzamutamanda ndi pakamwa panga mosalekeza . ” — Salimo 34 : 1 . Ndipo timapindula ndi maphunzilo oonjezeleka amene timalandila m’masukulu athu osiyanasiyana . Mukatelo , iwo adzaona kuti mumadalila Yehova . Abulahamu anapita kwa Sara ali wokondwela maningi . Izi zionetsa kuti palibe amene angazembe ciweluzo ca Yehova . 22 : 34 - 38 . M’bale woyamba kulalikila naye kunyumba ndi nyumba anali woyang’anila dela , amene pambuyo pake anadzaticezela . Mwacitsanzo , Yesu anacita pangano la Ufumu ndi ophunzila ake 11 okha , koma pangano limenelo limakhudza a 144,000 onse . Kukhulupilila zinthu zakuthambo monga nyenyezi , dzuŵa , mwezi , na mapulaneti , ni m’tundu winanso wa kuombeza . ( b ) Kodi buku lina linakamba ciani ponena za nthawi ya atumwi ? Izi n’zifukwa zocepa cabe zotsimikizila kuti Baibo imakamba zoona pamene imati : “ Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu , ndipo ndi opindulitsa pa kuphunzitsa , kudzudzula , [ na ] kuongola zinthu . ” — 2 Timoteyo 3 : 16 . Banja limeneli linali ndi ufulu wosankha lokha kudya zakudyazo kapena ai m’malo mokakamiza ena . Motelo , nchito imene Mulungu anapatsa Adamu idzakwanilitsidwa popanda iye . Felisa Ana ang’ono - ang’ono , kuphatikizapo azaka pakati pa 13 ndi 19 , amatengela kwambili makolo awo kuposa wina aliyense , ngakhale anzawo . Iwo anamponya miyala mobwelezabweleza cakuti iye anagwa pansi . Conco , Mose anauza Yehova kuti : “ Bwanji ngati sakandikhulupilila ndi kumvela mau anga ? Cifukwatu adzanena kuti , ‘ Yehova sanaonekele kwa iwe . ’ ” — Eks . Tilidi paubale weniweni . Ngati makolo apempha Mkhristu wina kuti aziphunzitsa ana awo coonadi , Mkhristuyo afunika kucita zinthu mosamala kuti asakhale ngati akulanda udindo wa makolo . Popeza tikukhala m’dziko limene limalimbikitsa ciwelewele , zingakhale zovuta kupewa mkhalidwe woipa umenewu . Iye ananena kuti : “ Panthawiyi ndimacita cidwi kwambili kuona maluwa akuphukila , mbalame zikubwelela kucoka kutali kumene zinapita , kuphatikizapo kambalame kakang’ono kooneka ngati kacoso ( kasongwe ) kamene kamabwela kudzadyela panyumba panga . Anadziŵanso kuti kukhala wophunzila kunali ndi mavuto ake . Kukulitsa cimwemwe tingakuyelekezele na kusonkhela moto . Ngakhale popanda kunyamula zida za nkhondo , Goliyati anali wolemela kuposa anthu aŵili akulu - akulu . Pamapeto pake , tidzakambilana mmene “ mtendele wa Mulungu ” ungatithandizile kupilila mavuto , tili na cidalilo conse mwa Yehova . Mulungu amadana na kuombeza kwa mtundu ulionse . M’Baibo timapeza mau aya : “ Pakati panu pasapezeke munthu . . . wolosela , wocita zamatsenga , woombeza , wanyanga , kapena wolodza ena , aliyense wofunsila kwa wolankhula ndi mizimu , wolosela zam’tsogolo kapena aliyense wofunsila kwa akufa . Nkhani yoyamba ionetselatu kuti Yehova ndi Mulungu wacikondi . Kapena tikukumana ndi mavuto ena obwela cifukwa cakuti tikukhala ‘ m’nthawi yapadela komanso yovuta . ’ ( 2 Tim . Zimenezi zidzatithandiza kuyambitsa maphunzilo ambili . ( Miyambo 3 : 12 ) Ngati timalola Yehova kutiphunzitsa ndi kulandila cilango cocokela kwa iye , timaphunzila kucita zabwino ndipo timakhala osangalala . Paulo anauza Timoteyo kuti : “ Gwila nchito ya mlaliki , ndipo ukwanilitse mbali zonse za utumiki wako . ” Kodi nikulola mtima wokonda zinthu zakuthupi kunilepheletsa kutumikila Mulungu modzipeleka ? Iwo anapangitsa anthu okhulupilika kuona masomphenya ocititsa cidwi . Eni nyumba imene tinali kukhalamo anabwela atakolewa , ndipo anayamba kuopseza kuti atipha . “ Seŵelo la Eureka , ” linakhala ciwiya cothandiza kwambili cimene Ophunzila Baibulo anali kugwilitsila nchito pophunzitsa anthu kuti anthuwo akaphunzitsenso ena atsopano . Iwo anati : “ Ungakonde kuyamba liti kuphunzila ? ” Zimenezi zingaoneke monga kuti zocita zathu zonse , ndi zimene zimaticitikila zinaikidwilatu . Tifunika kukonda miyezo ya Mulungu ndi kukhulupilila kuti ingatithandize paumoyo wathu . Kacisi ameneyu ndi dongosolo limene Yehova anakonza lotithandiza kukhala naye paubwenzi kudzela m’nsembe ya Yesu Kristu amenenso ndi wansembe . Yehova amathandiza atumiki ake kupilila mavuto aakulu Pamene Nehemiya anali kutsogolela Aisiraeli okhulupilika pa nchito yomanganso mpanda wa Yerusalemu , anakhazikitsa magulu a Alevi oimba na zida zoimbila . Monga mmene anali kucitila m’mbuyomo , atumwiwo anayambanso kukangana “ za amene anali kuoneka wamkulu kwambili ” pakati pawo . ( Ŵelengani 1 Akorinto 15 : 33 . ) Iye anati : “ Anthu kuno ali na cidwi ngako . 17 , 18 . ( a ) Kodi Yehova amafuna kuti akulu azisamalila bwanji nkhosa zake ? Kumeneku kungakhale kukaikila Mulungu Wamphamvuyonse . 28 : 13 - 15 . ) Nthawi zina , tingapeleke moni kwa ena mwa kumwetulila cabe kapena kuwakwezela dzanja . Kodi anthu a Yehova amaiona bwanji nkhani ya ulamulilo wake ? Kodi cikondi cimeneco cingasonyezedwe bwanji ? Mtumwi Paulo analemba kuti colinga ca Mulungu n’cakuti “ anthu kaya akhale a mtundu wotani apulumuke ndi kukhala odziŵa coonadi molondola . ” M’nthawi za m’Baibo kunalibe njila zamakono zotsogola zacipatala . ( Onani cithunzithunzi pacikuto . ) Fotokozani citsanzo ca mmene tingadzikonzekeletsele kudzakhala m’dziko latsopano . Ndani amene anali kudzakhala mbeu ? Nanga inali kudzatumikila pa udindo uti ? Acinyamata ndi acikulile akamayesetsa kulimbikitsa mgwilizano , ndiye kuti akukonzekela kudzapulumuka mapeto a dziko loipali lomwe mulibe mgwilizano . Nthawi zina , nayenso mtumwi Paulo anali kuvutika na cikumbumtima cifukwa ca zolakwa zake zakale . 22 : 9 . Anakavomela , sembe anali kusangalala ndi maceza ndi mfumuyo . Kupempha Citsogozo “ Ndiyendetseni m’njila ya malamulo anu , Pakuti ndikukondwela ndi njila imeneyi . ” — Salimo 119 : 35 . Abale ake anamvetsela maloto amenewo koma sanakondwele nao ngakhale pang’ono . Ndipo sanali kungoganizila zofuna zawo . Mtumwi Paulo anadziŵa mmene kufooketsedwa ndi zocitika za mumpingo ndi za kunja kwa mpingo kumakhudzila munthu . Akaziwo anali osiyana ngako na mkazi uja amene anatsekeledwa m’ciwiya copimila . M’zaka zimenezo , nthawi zina tinali kufooka mwauzimu . 3 : 1 , 13 ) Conco , tifunika kudzikonzekeletsa . ( 1 Timoteyo 5 : 8 ) Mungacite zimenezi osati mwa zokamba zanu cabe , komanso mwa zocita zanu . Nthawi imeneyi imaphatikizapo masiku 1,260 ( kapena miyezi 42 ) ndi masiku atatu ndi hafu ophiphilitsa ochulidwa pa Chivumbulutso caputala 11 . ( Miy . 19 : 20 ) Tikacita zimenezi , ndiye kuti ‘ sitinakane nzelu zopindulitsa . ’ Malemba amenewa amachedwa Septuagint . ( Danieli 7 : 13 , 14 ) Pokhala Mfumu , Yesu mtsogolo adzabweletsa mtendele padziko lapansi ndi kucotsapo njala . — Ŵelengani Salimo 72 : 7 , 8 , 13 . Ndipo timayamikilanso kusintha kokhudza misonkhano kumene kunapangidwa cifukwa kunatithandiza kuti tizikhala ndi nthawi yocita Kulambila kwa Pabanja ndi phunzilo laumwini . Rabeka ayenela kuti anali ndi mafunso ambili okhudza mmene umoyo wake udzakhalila m’dzikolo . Zitsanzo za m’Baibo zimaonetsa kuti kupeleka moni sikuthandiza cabe anthu kukhala omasuka , koma kumathandizanso m’njila zina zambili . 3 : 20 ) Mdyelekezi amafalitsa mabodza ponena za atumiki a Mulungu . N’cifukwa ciani kudziŵa mayankho a mafunso amenewa n’kofunika ? NWT ] ( Machitidwe 2 : 42 ) Anapitilizabe kukumana pamodzi ngakhale pamene anali kuzunzidwa ndi Boma la Aroma ndiponso atsogoleli acipembedzo aciyuda . Tikamaŵelenga mafanizo a Yesu tiyenela kudziŵa tanthauzo la mafanizo amenewo , cifukwa cake analembedwa m’Baibulo , cifukwa cake tiyenela kugwilitsila nchito mfundo zake , ndi zimene mafanizowo akutiphunzitsa ponena za Yehova ndi Yesu . Ngakhale n’conco , Yehova mwacikondi anatipatsa mabuku a Uthenga Wabwino amene amatithandiza kudziŵa bwino makhalidwe a Yesu . Genesis caputa 17 - 18 , 20 - 21 , 23 ; onaninso Aheberi 11 : 11 ; 1 Petulo 3 : 1 - 6 Tingacite zimenezi pamisonkhano pamene tipemphela kwa Yehova , kumuimbila , ndi kupeleka ndemanga . Liu lakuti nduna linagwilitsidwa nchito kwa Ebedimeleki , mnzake wa Yeremiya , ndi kwa mdindo wina wa ku Itiyopiya amene analalikidwa ndi mlaliki Filipo . Nchito yomasulila ndi kuphunzitsa imeneyi , ikucitika mobwelezabweleza m’zikhalidwe zosiyanasiyana . Mwacitsanzo : Tinene kuti mwapita pamalo odyela , ndipo akucenjezani kuti zakudya zonse pano ndi zosasa . Ophunzila Baibo okwana 8 amenewo anawaweluza kuti aikidwe m’ndende kwa zaka zambili ku Atlanta , Georgia . Posakhalitsa , tinayamba kucita phunzilo la buku ndi la Nsanja ya Mlonda wiki iliyonse m’cipinda cathu ca pa hotelayo , ndipo panali kupezeka anthu pafupi - fupi 15 . Iye monga mtumiki wothandiza , anapatsidwa nchito yosamalila maakaunti , mabuku ndi magawo . 1 : 47 ) Zocita zake . Kutalitali . Nthawi zambili kumabweletsa mavuto na kuwonongetsa miyoyo ya anthu . Iye amatikhululukila macimo athu , ndipo izi zimatithandiza kukhala osangalala . 25 : 15 . Mtumwi Paulo anacilitsa bambo wa Papuliyo amene anali kudwala malungo ndi kamwazi . Koma anthu oŵelenga Baibo mwakhama , amaona Cipilala ca Tito kuti cili na tanthauzo lalikulu kwambili . 41 : 8 ) N’ciani cinacititsa kuti munthu wokhulupilika ameneyu athe kukhala paubwenzi wolimba ndi Mlengi wake ? Pa Chivumbulutso 22 : 1 , 2 , mtumwi Paulo anakamba za “ madzi a moyo ” ndi “ mitengo ya moyo ” zimene zidzacilitsa anthu onse . Iyenso analephela kuyamikila colowa ca atate wake . 14 , 15 . ( a ) Kodi kukhala wokhwima mwauzimu kumaphatikizapo ciani ? Tidzaphunzilanso zimene atumiki anthawi zonse amacita masiku ano , ndi mmene tingawathandizile . Izi zinakhumudwitsa Akatolika , ndipo anayamba kulimbana ndi Mboni . Lomba nili na zaka zoposa 90 , ndipo nikali kutumikila monga mkulu mumpingo . ( Luka 17 : 10 ) Palinso mfundo ina imene tingaphunzilepo pa nkhani ya Hezekiya . Ataphunzila kuti Yehova alibe tsankho ndi kuti Satana ndiye amacititsa kuti anthu a mitundu yosiyana azidana , anayesetsa kuthetsa maganizo a tsankho . Abale Othandizila Makomiti a Bungwe Lolamulila Anthu akalosela amangoyembekezela kuti aone ngati zimene alosela zidzacitikadi . — Miyambo 27 : 1 . 6 : 12 ) Pa cifukwa cimeneci , tifunika kupewelatu “ zinthu zozikika molimba ” za m’dzikoli . N’cifukwa ciani mphatso ya Mulungu imaonetsa “ kukoma mtima kwake kwakukulu ” ? Ndipo alibenso cifundo ndi ana . Mtumwi Yohane analemba kuti : “ Mulungu anatisonyeza ife cikondi cake pakuti anatumiza m’dziko Mwana wake wobadwa yekha kuti tipeze moyo kudzela mwa iye . “ Tsopano ndazindikila cifukwa cake Yehova anakambila mau a pa Malaki 2 : 16 akuti : ‘ Ndimadana ndi zakuti anthu azithetsa mabanja . ’ Mwacitsanzo , magazini ya September 1 , 1895 , inati : “ Mbali imeneyi ya cilamulo ca Mose inali kucitila cithunzi citetezo cimene munthu wocimwa angapeze kwa Khristu . Popeza kuti ndinali kufunitsitsa kuphunzila , tinali kuphunzila kaŵili pamlungu , ndipo phunzilo lililonse linali kutenga maola pafupifupi anai . Izi zacititsa kuti cikhale covuta kwa iwo kulandila coonadi . Kodi mukugwilitsila nchito mokwanila zinthu zimenezi ? ( Mac . 10 : 45 ; Aroma 9 : 23 - 26 ) “ Mtundu woyela ” umenewu ni “ cuma capadela ” ca Yehova . Anthu a mu mtundu umenewu anadzozedwa na mzimu woyela komanso anasankhidwa kuti akakhale na moyo kumwamba . ( 1 Pet . Ojambula zithunzi ena amaonetsa Yesu ali wofooka thupi , wa tsitsi yaitali , na ndevu zing’ono kwambili kapena wa nkhope yacisoni . Tiyenela kuuza akulu pambuyo potsatila masitepe aŵili oyambilila , ndiponso ngati taona kuti munthuyo anatilakwiladi . Lekani nikusimbileni mbili yanga . Koma sitimalalikila cabe kuti tipewe mlandu wa magazi . Osati mphamvu zathu cabe , koma mzimu wa Mulungu . N’ciani maka - maka cimene acicepele angacite kuti asagonje polimbana na Mdyelekezi ? Mau a Mulungu amati : “ Kukongola kwa anyamata ndiko mphamvu zao , ndipo ulemelelo wa anthu okalamba ndiwo imvi zao . ” — Miy . Maganizo athu onse anali pa kupeleka cakudya cauzimu kwa abale athu . Koma Yakobo na Yohane sanamvetsetse mfundo imeneyi . Pambuyo pophunzilako nchito , n’nayamba kuseŵenza pa kampani inayake m’tauni yathu . Tidzadziŵa kuti aliyense wa iwo akali kuumbidwa . Iye anati , “ Kuŵelenga buku la Yobu kunandilimbikitsa . Okwatilana amalimbitsanso cikwati cao mwa njila ina akamauzana mau acikondi . Nyimbo youzilidwa ya Debora ndi Baraki imati : “ Kufikila pamene ine Debora ndinauka , kufikila pamene ine ndinauka monga mai mu Isiraeli . ” 9 UMBONI WINANSO 55 : 11 . Ndiye cifukwa cake Baibo inali yosoŵa ngati nyanga yagalu , titelo kukamba kwake , ndipo mtengo wake unali woboola m’thumba . Koma m’dziko latsopano limene likubwela , mudzakhala anthu ofatsa ndi olungama okha - okha . Ndi anthu otani amene tiyenela kupewa kugwilizana nao ? Inu makolo , mumacita mbali yaikulu yothandiza ana anu kukula kuuzimu . N’ciani cidzatithandiza kupulumuka panthawi imene anthu a Mulungu adzaukilidwa ? Atumiki a Yehova amafunikanso kukhala oona mtima osati odyela masuku pamutu anzao . Babulo Wamkulu , umene ndi ufumu wa dziko lonse wa cipembedzo conama , adzakhala woyamba kuonongedwa . ( Yes . 24 : 14 ) Mukatsatila malangizo amenewa , mudzayamba kuimba mokweza , mwamphamvu , na momasuka . Ngati ndife odzicepetsa , tidzazindikila kuti tilibe ulamulilo wonse . Pambuyo pochula amuna ndi akazi osiyana - siyana okhulupilika , Paulo anaunika citsanzo copambana onse — Ambuye wathu Yesu Khiristu . Abulahamu anali kukhulupilila kwambili malonjezo a Mulungu cakuti zinali ngati akuwaona akukwanilitsidwa . Ndimaona kuti io amafuna kudziŵa mavuto anga ndi kuti amandiganizila . Caciŵili , mwa zimene anali kuphunzitsa komanso citsanzo cake , Yesu anathandiza ophunzila ake kuona kuti nawonso afunika kupewa kukayikila ena kapena kuwasala . Conco , anapanga ulendo wina wa umishonale . Monga mmene anthufe timacitila nthawi zambili , mwina Aisiraeli anali kudziyelekezela ndi munthu woopsa ameneyu , ndipo anali kuwopa poona kuti anali kulekeza cabe m’ciuno mwake kapena pa cifuwa cake . Kucokela nthawi imeneyo , tinayamba kukumana nthawi iliyonse tikapeza mpata , koma tinali kucita izi mobisa . Riana anati : “ Nimaona kuti n’napanga cosankha cabwino ngako . ” ( Machitidwe 10 : 34 , 35 ) Maphunzilo amene Ufumu wa Mulungu ukupeleka kwa anthu padziko lonse lapansi angakuthandizeni kudziŵa zimene mungacite kuti mukhale nzika ya Ufumuwu . M’Baibulo , muli zitsanzo zambili za mapemphelo aciyamiko monga ya Hana ndi Hezekiya . ( 1 Sam . 2 : 1 - 10 ; Yes . Mu 1938 , Jim Carr , amene anali mtumiki wadela ( tsopano timati woyang’anila dela ) anathandiza kupeza nyumba zokhalamo apainiya m’mizinda . Kenako mu 1919 , zinali ngati kuti anthu a Mulungu akhalanso amoyo ndipo apatsidwa dziko latsopano . Kodi Rahabi anamuona bwanji Yehova ndi anthu ake ? Kodi Mulungu anadzoza Yesu kuposa “ mafumu ena ” m’njila zotani ? ( b ) Kodi tiyenela kucita ciani ngati tayamba kudzikonda ? Kudziŵa zimenezi kumatithandiza kuzindikila njila yabwino imene tingatsatile pa umoyo wathu kuti tikakhale na mtendele wosatha na umoyo wokhutilitsa m’tsogolo . Mtumwi Paulo anakamba kuti Akristu ali ngati anthu ocita mpikisano wothamanga . Kuti apambane mpikisano umenewu , io ayenela kucotsa ciliconse cimene cingawabweze m’mbuyo kapena kuwalepheletsa kuthamanga . ( Mateyu 5 : 27 - 29 ) Ophunzila a Yesu anali kukhala pakati pa Aroma amene anali kukonda kucita zaciwelewele , ndi kuonelela maseŵela a zamalisece amenenso munali mau oipa . Nyumba imeneyo iyenela kuti inali kacisi amene anamangidwa pofuna kulemekeza Mfumu ya Roma yochedwa Tiberiyo . 15 : 17 ) Ngati muika maganizo anu onse pa kucita cifunilo ca Yehova , iye adzakusamalilani panthawi ya ukalamba . Iye analangiza ophunzila ake kuti : “ Pitani ndi kulalikila kuti , ‘ Ufumu wakumwamba wayandikila . ’ ” ( Mat . Motelo Paulo anauza Timoteyo kuti : “ Pobwela utengenso Maliko , pakuti iye ndi wofunika kwa ine cifukwa amandithandiza pa utumiki wanga . ” — 2 Tim . Nthawi zina , akulu angaone kuti n’zovuta kutifikila kuti atipatse uphungu umene tikufunikila . Mulungu atalenga mwamuna woyamba Adamu , anam’patsa nchito yopatsa maina vinyama . NYIMBO : 88 , 115 8 Tumikilani Yehova , Mulungu wa Ufulu Masiku ano , mabanja amenewo amasangalala kwambili akakumbukila mmene anathandizilana panthawi ya mavuto . “ Nikapemphela kwa Mulungu , mzimu wake umanipatsa mphamvu . ” — Luis Conco , athandizeni kuti azikonda kuphunzila za Yehova ndi kudziŵa kuti kucita zimenezo kungawathandize kukhala anzelu . Iye waona kuti funso ndi mayankho patsamba loyamba zimathandizanso eninyumba kumasuka poyankha . Nowa , Danieli ndi Yobu anakumana na mavuto ambili monga amene timakumana nawo masiku ano . Iwo anapitiliza kusuliza uphungu wa akulu . Apa mfundo ni yakuti kuyamikila cisomo ca Mulungu kumafuna zambili kuposa kupewa cabe cigololo , kukolewa , kapena macimo ena amene anthu a ku Korinto anali kucita . Baibo imeneyo inali kuchedwa kuti Derekh ha - Kodesh , kutanthauza “ Msewu wa Ciyelo . ” Mau amenewo anacokela pa Yesaya 35 : 8 . Wamasalimo anapitiliza kukamba kuti : “ Mau anu amatsekemela m’kamwa mwanga , kuposa mmene uci umakomela ! ” ( Sal . 8 , 9 . ( a ) Kodi cikumbumtima cathu cimatithandiza bwanji ? 3 : 16 ) Conco , tifunika kumaŵelenga Baibo mwakhama , kusinkha - sinkha zimene imakamba , na kuziseŵenzetsa mu umoyo wathu . Tikatelo , tidzaphunzitsa cikumbumtima cathu kuti cizititsogolela mogwilizana na maganizo a Mulungu . Pafupi ndi iye panali Kora ndi anthu ake okwanila 250 , naonso atanyamula zofukizila nsembe . ( Num . Komabe , iye anali kupita kunyumbako mobwelezabweza . Cikwati m’nthawi imeneyo , kuphatikizapo cipali , cinatsogoleledwa ndi Cilamulo ca Mose . * Mumadziŵanso kuti pafunika abale ambili amene angalimbitse mipingo imene ilipo ndi kukhazikitsa mipingo ina yatsopano . 28 : 19 , 20 ; 1 Pet . Iye anati : “ Sin’nali kudziŵa kumene nidzapita kukatumikila , utumiki umene nidzacita , kapena mmene nidzaucitila . Cifukwa cakuti tinapangidwa m’cifanizilo ca Mulungu , timakonda cilungamo . Conco malamulo amene maboma a anthu amapanga nthawi zina angatikhumudwitse . ( Gen . 1 : 27 ; Deut . Anali kudziŵa kuti Yehova sangacite zinthu mopanda cilungamo mwa “ kupha olungama pamodzi ndi oipa . ” ( Miy . 28 : 13 ) Koma kubisa chimo n’kusoŵa cikondi cifukwa sikuvulaza cabe wolakwayo , koma kumavulazanso Akhristu ena . ( Yoh . 17 : 3 ) Kuti ana anu aphunzile mfundo za Yehova , mufunika ‘ kumalankhula nawo ’ za mau ake pa mpata uliwonse woyenelela . — Ŵelengani Deuteronomo 6 : 6 , 7 . Kuti mudziŵe zambili zimene Baibo imakamba ponena za angelo okhulupilika ndi osakhulupilika , onani nkhani 10 m’buku la Zimene Baibulo Ingatiphunzitse lofalitsiwa na Mboni za Yehova . Ganizilani izi : Pamene anali kumwamba , Yesu anaona Yehova akuyankha mapemphelo a atumiki Ake pano padziko lapansi . Mwacitsanzo , yelekezelani kuti mukusamalila wacibale wanu amene akudwala matenda aakulu . Anthu amene ali na zolinga zadyela sapeza cimwemwe cimene amafuna . Dipo ndi umboni wakuti Mulungu amakonda anthu . ( Yoh . Kodi oukitsidwa padziko lapansi “ sadzakwatila kapena kukwatiwa ” ? ( Onani ndime 21 ) Pamene ndinafika zaka 18 , zinandivuta kusankha kuti ndipite ku univesite , ndiloŵe nchito , kapena kucita upainiya . Iye amamva monga mmene Mfumu Davide anamvelela pamene anakamba kuti : “ Ndimakondwela ndi kucita cifunilo canu , inu Mulungu wanga , ndipo cilamulo canu cili mumtima mwanga . ” ​ — Salimo 40 :⁠ 8 . Koma zina zimene anali kukambitsilana sin’nali kuzimvetsetsa . Conco , zinadzipeleka kuti zikonze . Patapita nthawi , munthuyo analemba kalata ku likulu la Mboni za Yehova . Mkalatayo anati : “ Niyamikila kwambili thandizo lanu . Iwo afunika kuonetsana cikondi cacikulu monga mmene Abulahamu ndi Sara , Isaki ndi Rabeka , komanso Elikana ndi Hana , anacitila . Anthu amene ali na cuma koma sangakwanitse kucita utumiki wa nthawi zonse kapena kusamukila m’dziko lina , amakondwela podziŵa kuti zopeleka zawo zimathandiza ena amene akucita utumiki . ( Miy . N’nakondwela kwambili cifukwa n’nakwanitsa kubweza mkwiyo wanga . Ganizilani zimene mukanakonda kuti ena akucitileni ngati munali mumkhalidwe wofanana ndi umenewo . Pa zosankha ngati zimenezi , tifunika kudalila Yehova kuti atitsogolele ndi kutipatsa malangizo abwino amene angatithandize . Komabe , si onse amene amamvetsela uthenga wathu tikawalalikila . ( Yoh . Alimiwo anacita zinthu zofanana na zimene Aisiraeli anacita , amene anazunza aneneli a Mulungu otumiziwa kwa iwo . Munthu akapita patsogolo n’kuyamba kutumikila Mulungu , amabala zipatso m’njila yakuti amadzipeleka kwa Yehova n’kubatizidwa . Ndithudi , galetayi ili paliŵilo ! Pamene Paulo anali kulemba zimenezi , anali kukamba za abale amene anali m’ndende cifukwa ca cikhulupililo cao . 8 , 9 . ( a ) Ni cenjezo lanji limene mtumwi Petulo anapeleka pa nkhani yoseŵenzetsa ufulu wathu ? Nthawi imeneyo inali yosangalatsa ngako . Koma ambili mu mpingo wathu anali kukamba Cikigizi . Patapita masiku anai Lazaro ali m’manda , Yesu anafika ku Betaniya kuti akatonthoze Marita , mlongosi wa womwalilayo . OPEZEKA PA CIKUMBUTSO ( 2015 ) Koma lemba la Chivumbulutso 11 : 7 - 12 , limanena za kagulu kocepa ka abale odzozedwa amene akhala akutsogolela anthu a Mulungu . NYIMBO : 93 , 96 VUTO : M’maiko ambili mumacitika masankho nthawi ndi nthawi . Anatiŵelengela buku lakuti , Kucokera ku Paradaiso Wotaika Kumka ku Paradaiso Wopezedwanso . Koma posacedwapa , tinaona kuti m’poyenela kusintha mmene timafotokozela ulosi umenewu . Conco , iye na mwamuna wake anaganiza zotenga mwana wa anthu ena kuti azimulela monga wawo . 2 : 21 ) Pamene analemba zimenezi , Paulo anali ku Roma . Mwacitsanzo , ngati muli pamwamba pa phili lalitali kapena m’ndeke , anthu ndi zimene iwo anapanga zimaoneka ngati zacabe - cabe . Citsanzo cina ndi ca Ndenguè wa ku Cameroon . Ndipo mwana wake anati : “ Ndicitileni mogwilizana ndi zimene zatuluka pakamwa panu . ” 12 : 3 ; Sal . 106 : 32 , 33 ) Ndiponso , m’bale ‘ sangadziŵe kanthu kalikonse kum’tsutsa mumtima mwake , ’ koma ena angadziŵe zofooka zake . ( 1 Akor . Mulungu analonjeza kuti : “ Ine ndi amene ndimanena za mapeto kuyambila pa ciyambi . . . Tiyeni tionenso citsanzo cina . Kuyamikila malo athu mu utumiki wathu kwa Yehova kudzatithandiza kucita zimenezi . M’malo mofuna malo apamwamba kapena kufuna kumatenga malo a ena , tizifunsila kwa ena ndi kumvela maganizo awo . ( Miy . ( Media and Society in the Twentieth Century ) . Komabe , akatswili a Baibulo anapenda mosamalitsa mipukutu yambilimbili ya Baibulo ndi Mabaibulo ena akale . Iwo anadzipeleka kwa Atate wawo wakumwamba , Yehova , ndipo kucita cifunilo ca Mulungu ndiye cinali cinthu cofunika kwambili pa umoyo wawo . Tinali kucomelela , conco anali kutipatsa cakudya ca masana . Pamene anthu a mu ufumu wa Isiraeli wa mafuko 10 wolamulidwa na Yerobowamu anayamba kulambila mafano , anthu ambili ocokela kumeneko ‘ analimbikitsa Rehobowamu . ’ Nthawi zina ndimawatumizila tumphatso tung’onotung’ono . 48 : 17 . 1 : 26 , 27 ) Pambuyo poti Yehova walenga munthu woyamba , Adamu , Iye anam’patsa mkazi wokongola . Kodi mukumbukila mmene amayi anu anakutonthozelani ? Komabe , cifukwa cakuti ndife osiyana , nthawi zina timasemphana maganizo . Sanali kungouza mwamuna wake zom’komela m’khutu ayi . 100 : 2 ) Nanga tingalalikile bwanji uthenga wabwino mogwila mtima kwa anthu othaŵa kwawo amene sadziŵa Yehova ? Iwo amathandiza mpingo kukhala wolimba . Kukhala na cikhulupililo colimba tingakuyelekezele na mmene maluŵa amafunila madzi . Mulungu woona anapatsa mbeu ya mkazi wakumwamba mphamvu yoononga Satana . Iwo anali kungopemphela kwa Yehova kuti atumize m’bale amene ali na mpeni . Toby ali na zaka 12 , anadziikila colinga coŵelenga Baibo yonse yathunthu akalibe kubatizika . ( Luka 7 : 22 ) Yesu anafika ngakhale popeleka moyo wake pofuna kuwombola mtundu wa anthu . Komanso tifunika kuucilikiza na mtima wonse . Ndiyeno Yesu anamuuza zinthu zimene zinali kuoneka ngati zosatheka , anamuuza kuti anyamule macila ake ndi kuyamba kuyenda . Inunso mungakwanilitse zolinga zanu zauzimu . Ngati tingabwezele mwanjila ina iliyonse , ndiye kuti sitikulemekeza Yehova . Yehova amakonda anthu ake osati monga gulu cabe , koma amakondanso aliyense payekha . N’ciani cingacititse ena kukaikila ngati Mulungu amawasamaliladi ? Kodi Davide akanakhala ndi moyo masiku ano , akanamva bwanji kuona nchito yaikulu yomanga imene ikucitika ? ▪ Baibulo Lomasulidwa Bwino Kwambili Dale , katswili wa zomangamanga , ndi mkazi wake Cathy , a ku Alabama , amayamikila kwambili utumiki umenewu . Lembali linalembedwa zaka zambili Paulo atalembela kale Timoteyo makalata . Kodi zocitika zimenezi zitiphunzitsa ciani ? Zimene Anthu Acita Pofuna Kugonjetsa Imfa Tikamacita zimene timaphunzila , timakhala na umoyo wabwino ndipo cikhulupililo cathu cimalimba . — Aheberi 11 : 1 . “ Mafunso opusa ndi opanda nzelu ” anaukhudza bwanji mpingo wacikristu woyambilila ? Lemba la Machitidwe 2 : 5 - 11 lionetsa kuculuka kwa anthu amene anapezeka pa Pentekosite mu 33 C.E . Wolemba nkhani wina waciyuda , dzina lake Philo , anatsimikizila zimenezi . Taphunzilapo kuti ndi udindo wathu kupanga zosankha . Koma kuti zosankhazo zikhale zanzelu zifunika kuzikidwa pa cidziŵitso colongosoka ca m’Malemba . Ngakhale ndi conco , angelo okhulupilika amagwilitsila nchito mphamvu zao pocita zinthu zabwino . Kukonda ulamulilo wa Mulungu na kulemekeza mfundo zake zabwino , n’zinthu zofunika kwambili zimene inu makolo muyenela kuphunzitsa ana anu . — Ŵelengani Miyambo 1 : 5 , 7 , 8 . Imeneyi ni mfundo yolimbikitsa kwambili . Kodi pakati pa Aisiraeli panali dongosolo ? Fotokozani . Iwo akuonanso mavuto amene mukukumana nao , koma akukucemelelani kuti musagonje . Ninayankha kuti “ Inde , ” ngakhale kuti n’nali n’kalibe kulalikilapo . 8 : 6 ; 9 : 15 . ( Chivumbulutso 12 : 9 , 12 ) Conco , Satana Mdyelekezi ndiye amacititsa mavuto ambili . 12 : 9 ) Mayeselo amene takumana nawo alimbitsa cikhulupililo cathu ndi kutithandiza kukhalabe okhulupilika . ( Sal . 72 : 13 ) Ndithudi , Yesu mofunitsitsa adzathandiza anthu ovutika . ya July 2010 , tsamba 8 . Tiyenela kulimbitsa ubwenzi wathu na Yehova mwa kuŵelenga Baibo na kugwilizana kwambili na anthu odzipeleka potumikila Yehova . Tili na mwayi wopemphela kwa Mulungu . Izi zionetsa kuti Mlembi wake weni - weni ni Mulungu wamphamvuzonse . ABUSA m’nthawi ya Isiraeli wakale anali ndi nchito yovuta kwambili . ( Ower . 6 : 36 - 40 ) Ngakhale kuti Gidiyoni anali munthu wolimba mtima , anacitabe zinthu mosamala ndi mwanzelu . ( Ower . M’nthawi yocepa , mfundo zoyambilila za m’Malemba zimene anaphunzila ndi kuziyamikila , zinam’sonkhezela kuti abatizike . Mnzanga mmodzi , dzina lake Gust Maki anali kaswili woyendetsa boti . Mulungu Anamucha Mfumukazi Iye anali na ulamulilo waukulu , koma anapewa kuugwilitsila nchito molakwika pamene anali kuvutitsidwa na Sauli ndi pamene ananyozedwa na Simeyi . ( 1 Sam . 26 : 9 - 11 ; 2 Sam . Ngakhale kuti Yehova anapulumutsa Aisiraeli ku Iguputo , Gidiyoni panthawiyi anakaikila ngati Yehova adzawathandizadi . 15 , 16 . ( a ) N’cifukwa ciani ena amanyalanyaza kuyeletsa pa Nyumba ya Ufumu ? M’Baibulo muli mau ocepa a Yesu amene analembedwa m’cinenelo ceniceni cimene iye anali kukamba . ( a ) Kodi kuyamikila dipo kuyenela kutisonkhezela kucita ciani ? Ngakhale Akristu ena asankha zinthu zoipa ndipo cifukwa ca kucita zinthu “ mwacinyengo , ” awononga mbili yawo mumpingo . — 1 Timoteyo 3 : 8 ; Tito 1 : 7 . 10 : 12 , 13 ) Pamene mukali acinyamata , pangani cosankha cimene cidzakuthandizani kukonda Yehova ndi kum’tumikila “ ndi mtima wanu wonse , ndi moyo wanu wonse . ” M’nzake wa Jairo , Alex anati : “ Nthawi zonse ndimalimbikitsidwa ndikamva Jairo akupeleka ndemanga pa nkhani ya m’Baibulo . ” Komanso , Mau ake amakamba kuti “ iye amakonda cilungamo ndi ciweluzo cosakondela . ” — Sal . Asanamangidwe , Dr . ( Chivumbulutso 22 : 17 ) Koma tingathe kucita zimenezi ngati ndife ‘ olumikizana bwino , ’ ndiponso ngati ticita zinthu mogwilizana mumpingo . — Aefeso 4 : 16 . Mapeto ake , anacita ngozi yoopsa , titelo kukamba kwake . Anadzibweletsela ucimo na imfa , ndipo zimenezi zinafalikila kwa mbadwa zawo zonse . Mau akuti “ paladaiso wauzimu ” timawagwilitsila nchito kwambili m’gulu lathu . Motelo , angadzifunse kuti , “ Kodi n’kwanzelu kuganizila kuti ndingapeze munthu wondikwatila mumpingo ? ” Ngati munakhalapo ndi maganizo amenewa , dziŵani kuti Yehova amadziŵa za vuto lanulo ndi mmene mukumvelela . — 2 Mbiri 6 : 29 , 30 . 4 : 7 - 10 . Kodi anthu amene apanga khamu lalikulu acokela kuti ? Komanso sanali kudela nkhawa za cakudya , matenda , na imfa . Analinso na nchito yabwino . ( Gen . Pokambilatu za anthu ake a m’tsogolo , Mulungu anati : “ Ndidzawabweletsa pamalo amodzi ngati gulu la nkhosa m’khola . ” N’zoona kuti sitidziŵa zonse zimene Yehova adzacita panthawiyo . Koma panganoli linayamba kugwila nchito mu 1943 B.C.E . , pamene Abulahamu anali ndi zaka 75 , anacoka ku Uri ku Mesopotamiya , ndi kuoloka Mtsinje wa Firate . 4 : 1 - 3 , 13 ; 5 : 6 - 8 . * ( Genesis 17 : 17 ) M’kupita kwa nthawi , Abulahamu anachedwa “ tate wa onse . . . okhala ndi cikhulupililo . ” Ndipo Yesu anati : “ Musaope , kagulu ka nkhosa inu , cifukwa Atate wanu wavomeleza kukupatsani Ufumu . ” Koposa zonse , ulaliki wa Yesu unapeleka ciyembekezo ca moyo wosatha kwa anthu omumvetsela . Zinali zovuta kwambili kuti munthu aphunzile coonadi kapena kuti aphunzitse wina . ( Mateyu 24 : 21 ) Koma kumeneku si kutha kwa Dziko cifukwa ca zocita za anthu kapena ngozi za cilengedwe . Colinga ca Mulungu n’cakuti dziko lapansi likhalepo mpaka kalekale . Tinayamba kukangana ndi mkazi wanga cifukwa cosoŵa ndalama . Amakamba kuti : “ Cinalembeka kale kuti sinizakwanilitsa ! ” Kodi Mulungu amakuŵelengelani ? N’ciani cimatisonkhezela ‘ kucenjeza anthu oipa kuti asiye njila zao zoipa ’ ? ( Mlaliki 3 : 7 ) Pali nthawi yotamanda Yehova , yolimbikitsa ena , yokamba maganizo athu , ndi youza ena zimene tikufuna . Zikuoneka kuti cimoto coopsaco cinayamba cifukwa ca tumalaŵi twa moto tocoka m’sitima imene inali kudutsa m’nkhalangoyo . Umenewu ndi mwai umene tiyenela kuyamikila . 40 : 7 , 8 ) Yesu anadzipatulila kuti acite cifunilo ca Yehova , olo kuti anali wobadwila mu mtundu wodzipatulila kale kwa Mulungu . “ Tizisonyezana Cikondi Ceni - ceni m’Zocita Zathu , ” Oct . Lelo lino , pali abale ambili amene akangalika pamaudindo kwa zaka zambili , ndipo akonzekeletsa acinyamata kutenga maudindowo . ( 1 Mbiri 22 : 7 ) Iye anali kufunitsitsa kumanga nao kacisi amene anali kudzapeleka ulemelelo kwa Mulungu . Kodi cikumbumtima cophunzitsidwa bwino cingatithandize bwanji popanga zosankha ? Cifukwa Baibulo limati kutaya cikhulupililo “ ndi chimo limene limatikola mosavuta . ” David : Zoonadi , monga mmene Gwen wakambila , zolinga zathu zinaticititsa kukhala ndi mwai wokavinila m’nyumba yaikulu yocitilamo maseŵela ya Royal Opera House ( nyumbayo masiku ano imachedwa English National Ballet ) komanso kukhala m’gulu lina la ovina lochedwa London Festival Ballet . Kodi timaonetsa bwanji kuti timayamikila dipo ? Kodi mumamva bwanji kukhala ndi zinthu zimene munalandila ? Tinafunsa akulu amene atumikila kwa zaka zambili ocokela m’maiko 20 a azungu kuti atiuze cifukwa cake abale acinyamata amakana maudindo mumpingo . Conco Goliyati anafuula kuti : “ Kodi ine ndine galu kuti ubwele kwa ine ndi ndodo ? ” Yehova anamukwiyila kwambili Mose . ( Deut . Kodi anacita ciani ndi lonjezo la atate wake ? Kucita zimenezi kumatigwilizanitsa ndipo timakhala ndi zambili zodzasimba mtsogolo . Dipo ndiye njila yaikulu imene Mulungu waonetsela cikondi cake m’mbili yonse ya anthu . Komabe , n’kulakwa kuganiza kuti ngati mwana sanabatizike , ndiye kuti Yehova sangamuŵelengele mlandu akacimwa . N’cifukwa ciani tingadabwe kuti Mose anataya mwayi woloŵa m’Dziko Lolonjezedwa ? Zimenezi zimandicititsa kumvetsa bwino coonadi . ” Mwacibadwa , iye anali munthu wansangala ndi wolimba mtima . Farao anapatsanso Yosefe cheni cagolide , mphete yacifumu , galeta laciŵili laulemu , ndi ulamulilo wopita kulikonse m’dzikolo kukagwila nchito yake yosonkhanitsa cakudya . Tiyelekeze kuti mwapempha m’bale kuti ayeletse pakhomo la nyumba ya Ufumu ndi kukonza zinthu zimene zingapangitse ngozi . Yesu monga mphunzitsi , anali kuwafika pamtima anthu cifukwa cokonda Yehova , Mau a Mulungu , ndi anthu . ( Luka 24 : 32 ; Yoh . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Tikanena kuti : ‘ Tilibe ucimo , ’ ndiye kuti tikudzinamiza . ” — 1 Yohane 1 : 8 . Colinga ca Yehova cokhudza mtundu wa anthu omvela cikuonekela bwino m’pemphelo la citsanzo la Yesu . YEHOVA sanafune kuti anthu azivutika ndi ukalamba . Pamene oweluza aciisiraeli anali kutsatila miyezo ya pamwamba imeneyi , mtundu wonse unali kuona kuti ndi wotetezeka . Ndiye cifukwa cake nthawi zambili timalimbikitsidwa kuti tiziŵelenga Baibo tsiku lililonse . ( Sal . Sanawacitenso macimowo . Nili kumeneko , n’nacita cidwi ngako ndi ana . Kulimba mtima kwa Yosefe pofuna kucita cilungamo , kunacititsa Yakobo atate ake kumupatsa mphatso yaulemu . Kodi Yehova amayang’ana ciani mwa atumiki ake ? N’zosadabwitsa kuti m’kupita kwa nthawi , Timoteyo anakhala woyang’anila wabwino wacikristu . ( Afil . Yehova amadziŵa zimene zidzacitika mtsogolo , ndipo amatiuzilatu zimenezo kudzela m’Malemba . Ndikusangalala ndi banja langa ndipo ndikutumikila ndi cikumbumtima coyela cifukwa ndikutsimikiza kuti Yehova anandikhululukila . Pa cocitika cina , nduna ya ku Itiyopiya inali kuŵelenga mbali ina ya m’Malemba . Timakhala titatsitsimulidwa , ndiponso timakhala na mphamvu zotithandiza kupilila mavuto amene timakumana nawo . Eduardo anayesetsa kucita zonse zimene akanatha kuti ayambenso kugwilizana ndi banja lake ndi kulithandiza kuuzimu . Mu July 1956 , tinatsiliza Sukulu ya Giliyadi ya namba 27 . Ndiyeno , mu November tinayamba utumiki wathu ku Brazil . Tinawathandiza kukhala na zolinga zoyamba utumiki wa nthawi zonse ndi ubwino womanga banja na munthu wofanana naye zolinga . Anali kugaŵila magazini ambili - mbili pamwezi . Musaleke kucita zimenezo . Abale ena amene atumikila pa Beteli amagwila nchito yopulinta ndi kukonza Mabaibulo ndi zofalitsa zina . 25 : 8 ) Umphawi adzauthetsa . Sindinakaŵelenge kapepalako cifukwa ndinali kuona kuti mabuku a conco amaoneka kuti ali ndi coonadi pamene alibe . Ngakhale zinali conco , tinapitilizabe kuyendela mipingo mpaka mu 1967 pamene boma la Malawi linaletsa cipembedzo ca Mboni za Yehova . Inu Yehova ndinu Mulungu wathu . Nanga mungacite ciani kuti mavalidwe anu azilemekeza Mulungu ? Zinthu zonse zimene ndikupanga n’zatsopano . ” — Chivumbulutso 21 : 4 , 5 . Komabe , n’kayamba kuganiza conco , n’nali kukumbukila mau amene Petulo anauza Yesu akuti : “ Ambuye , tingapitenso kwa ndani ? Yehova angatipatse mphamvu kuti tipitilize “ kugonjetsa coipa mwa kucita cabwino . ” Pano , Aaron ni mkulu ndipo atumikila pa Beteli . Baibulo imakamba za anthu ambili amene anakhalabe okhulupilika kwa Yehova ngakhale kuti anthu amene anali kukhala nao anacita zolakwa zazikulu . Conco , n’nauzidwa kuti nizigwila nchito imene iye anali kucita , ndipo n’nayamba kutumikila pamodzi ndi m’bale Don Adams . Kuti tisabwelele m’mbuyo pogwila nchito yolalikila imene Yesu anatipatsa , tiyeni tikambilane mafunso aya : N’cifukwa ciani nthawi zina tikhoza kulefuka pogwila nchitoyi ? Mukagwilitsila nchito Mau a Mulungu kudziyesa kuti ‘ muone ngati mukali olimba m’cikhulupililo , ’ mudzayamba kudziona monga mmene Mulungu amakuonelani . Cipembedzo ndi cikhalidwe ca Akanani cinali cankhanza , anali kupeleka ana nsembe ndipo anali kucita ciwelewele pakacisi . Ndiponso , kukhala ndi cizoloŵezi cokaikila kukhulupilika kwa ena mu mpingo kungaononge ubwenzi wathu ndi Yehova . Tingayambe kudziona ife eni , kapena utumiki wathu monga ndiye wofunika kwambili . Koma pali pano , timacita zonse zimene tingakwanitse kuti tithandize amene akukumana ndi mavuto amenewa . Ngati simukamba zoona , mwamsanga anthu adzaleka kukudalilani . Cifukwa coseŵenzetsa liu lakuti “ ndiyeno ” pa vesi 12 , tsopano madalitso ochulidwa m’mavesi 12 mpaka 14 amamveka kuti ni opita kwa olungama , amene anapempha kuti ‘ amasulidwe ndi kulanditsidwa m’manja mwa anthu ’ oipa ( vesi 11 ) . Koma makhoti anakana , ndipo ine n’naweluzidwa kuti nikakhale m’ndende masiku 31 . Pamene Akhiristu ateteza cikhulupililo cawo pamaso pa mafumu , abwanamkubwa , kapena akulu - akulu a boma , amakhala kuti akulalikila anthu amene mwina sizikanatheka kuwalalikila . Kodi muyenela kukhala ndi colinga cotani pamene mukuphunzila Mau a Mulungu ? ( b ) Timadziŵa bwanji kuti n’zotheka kupambana polimbana ndi Satana ? Mungaganizilenso zolinga zina zimene mungakwanitse . ( Genesis 9 : 1 - 4 ) Lamulo limeneli limatithandiza kudziŵa mmene Mulungu amaonela moyo . Zimenezi zinalidi zolimbikitsa kwambili cifukwa m’baleyo anali ndi banja , koma anadzipeleka ngakhale kuti sanali kudziŵa kumene azidzapeza ndalama zosamalila banja . Wosimba ni Walter Markin 1 : 20 . Moimilako Yehova , Mose mtsogoleli wa mtundu wa Isiraeli wakale , anauza anthuwo ali pafupi kungena m’Dziko Lolonjezedwa kuti : “ Ndaika moyo ndi imfa , dalitso ndi tembelelo pamaso panu . . . . Komabe , iye amateteza anthu ake monga gulu mwa kuwacenjeza za njila zosiyanasiyana zimene Satana amagwilitsila nchito kuti awasoceletse . YEHOVA ndiye Gwelo la nzelu , ndipo amagaŵilako ena nzelu zake mowoloŵa manja . Koma nthawi zina , cilango ca Mulungu cingapose pa uphungu kapena kuwongolela cabe . Davide anaona kuti Goliyati anali kunyoza Yehova . Kodi kugwila nchito ya Yehova nthawi zonse kungatithandize bwanji kuikabe maganizo athu pa nkhani yaikulu ? Kuti anthu a Mulungu akhale akapolo a Babulo Wamkulu mu 1918 , cipembedzo conama cinafunikila kuwatengela mu ukapolo mwa njila inayake panthawiyo . Ngati pali cinthu cimene tingacite kuti tikhale ndi moyo wokhutila , ndi kutumikila Yehova . Ngakhale kuti zimene iwo asankha ise sitinazikonde , tifunikabe kucilikiza dongosolo la Mulungu . Izi n’zosiyana ndi zimene anthu a m’dzikoli amacita . Mwacitsanzo , nkhani za mutu wakuti “ Zoti Muchite Pophunzira Baibulo , ” zimene zipezeka m’cigawo cakuti “ Achinyamata ” pa jw.org ( peji ya Chichewa ) , zingakuthandizeni kuphunzila zambili pa nkhani za m’Baibo . Nkhani ya m’Baibulo imeneyi imatikumbutsa kuti ngakhale kuti ndife opanda ungwilo , Yehova adzapitilizabe kutionetsa cikondi cake cosatha ngati timayesetsa kucita zinthu zom’kondweletsa . Kodi mungakonde kudziŵa zimene maulosi a m’Baibo amakamba zokhudza masiku athu ano ? Koma Yehova Mulungu wanibwezela zoculuka kuposa zimene napeleka . . . . Nanga bwanji ngati tili ndi nkhawa cifukwa cakuti moyo wathu uli pa ngozi ? Ukapolo umenewo unayamba pambuyo pa caka ca 100 C.E . , ndipo unatha m’caka ca 1919 . ( 1 Atesalonika 5 : 14 , 15 ) Akulu mumpingo ayenela kukhala citsanzo cabwino pankhani imeneyi . — Aefeso 4 : 8 , 11 - 13 . 5 : 1 ) Komabe , nthawi zina kuona mosayenela anthu ofunikila thandizo kungaticititse kuti tilephele kuwathandiza . Ngati Yesu sanaukitsidwe , cifuno ca Mulungu cikanalephela ndipo uthenga wabwino umene io anali kulalikila ukanakhala wopanda phindu . ( Luka 12 : 15 ) Ngakhale kuti nthawi zina tingaganizile zinthu zoipa , tiyenela kuongolela maganizo athu kuti zikhumbo zoipa zisatiloŵetse m’chimo . — Ŵelengani Yakobo 1 : 14 , 15 . Unanithandiza kukhala womasuka . Ndidzamuteteza cifukwa wadziŵa dzina langa . ” — SAL . “ Inu Yehova mwandithandiza ndi kundilimbikitsa . ” — Salimo 86 : 17 . Nikaganizila kale langa , nthawi zina nimaona kuti umoyo wanga ulinganako na wa mneneli Amosi . Kwabena wa ku Ghana , anakamba cifukwa cake anapempha Mulungu kuti amuthandize . Cangu canu cidzalimbikitsa abale anu ndiponso anthu amene mumalalikila . M’kupita kwa nthawi , cikhulupililo cao cinali kukulilakulila nthawi zonse akaona mmene Yehova anali kuwathandizila . Munthuyo anakamba kuti amafuna kukhala m’gulu limene “ sililekelela khalidwe loipa . ” Mwina mungaganize kuti nkhani zimenezi n’zazing’ono . Zinali zomveka iye kukhumudwa . Makolo anga anali kufuna kuti ndipite ku univesite n’colinga cakuti ndidzapeze nchito yabwino . ya July 8 , 2003 , mapeji 28 - 32 . Mofanana ndi Kaini , Mkhristu masiku ano angakambe kuti amalambila Yehova , koma n’kumacita zinthu zina zimene iye amazonda . Conco , tiyeni tiziyesetsa kupezeka pamisonkhano yonse . M’mawebusaiti amenewo mumapezeka zinthu zimene colinga cake ni kuyambitsa cikayikilo m’mitima mwa oŵelenga . Kodi ine ndatenga malo a Mulungu ? Thandizani mwana wanu kudzimva kuti mumam’konda mwa kumuuza nthawi zonse kuti , “ Ndimakukonda kwambili . ” Monique anapitiliza kuti : “ Nthawi yomweyo n’nazindikila kuti n’nalibe ndalama zokwanila , ndipo n’nali wosakonzekela kukukila ku dziko lina . ” Zimene limatanthauza ( Yohane 3 : 3 , 5 ) Kenako Yesu anati : “ Usadabwe cifukwa ndakuuza kuti , anthu inu muyenela kubadwanso . Iye anawathandiza kuwongolela maganizo olakwikawo mwa kuwafotokozela fanizo la ndalama za mina . Sitifunikila kucita manyazi cifukwa ca banja lathu , mtundu wathu , kapena dela limene tinakulilako . — Mac . 21 : 39 . Koma tinakumananso na mavuto ena aakulu kwambili . Sivulsky ) , Aug . Akristu a m’nthawi yakale anafunika kuyembekezela tsiku la Yehova , ndipo kucita zimenezi n’kofunika kwambili kwa ife masiku ano . Kuitanila ena ku cakudya : M’nthawi zakale , kaŵili - kaŵili anthu anali kuceleza anzawo mwa kuwaitanila ku nyumba kwawo kuti akadye nawo cakudya . ( Gen . 18 : 1 - 8 ; Ower . Pedro , wa ku South America , amene anasamukila ku Australia pamodzi na banja lake anati : “ Ngati munthu aphunzila zinthu zauzimu , amafunika kukhudzidwa mtima . ” — Luka 24 : 32 . Iye anapitilizabe kukonda Paulo . ( 2 Pet . Cikondi ceni - ceni cimadziŵikitsa Akhristu oona . N’kumenenso anali kulambila Mulungu wawo Yehova kwa zaka zambili . Yehova amadziŵa zimene zingatipindulitse . Palibe amene angafune kucita zimenezo . Nimaona kuti n’kanapitiliza khalidwe la conco , inenso sembe n’nafa kale . Iwo amaona kuti kukhala wacinyamata ndi wamphamvu , ndi pamene zinthu zingakuyendele bwino . 11 : 9 ) Komabe , masiku ano timaphunzilanso zambili . Conco , ganizilani za munthu amene mufuna kupatsa mphatso . Ndiye cifukwa cake m’Baibo amachulidwa kuti “ ana a Mulungu woona . ” — Yobu 1 : 6 ; Salimo 148 : 2 , 5 . Okwatilana sangathetse mavuto mwa kulalatilana kapena kuleka kulankhulana . ( 1 Mafumu 19 : 1 - 4 ) Ndi kuti kumene iye akanapeza thandizo ndi cilimbikitso ? Pamene tiimba nyimbozi , zimakhala ngati tikuuza Yehova za mumtima mwathu . ( Ŵelengani Aroma 14 : 4 . ) Fotokozani citsanzo ca kupanda cilungamo kumene kumacitika m’dzikoli . M’kanthawi kocepa , mliliwo unapha anthu ambili . N’taŵelenga kuti ‘ kwa anthu ambili , nkhondo yolimbana ndi zilakolako zoipa ndi yaikulu kwambili , n’naona kuti sinili nekha . ” 3 : 9 - 12 . Koma misonkhano yathu imatilimbikitsa ndi kutipatsa mphamvu kuti tipitilize kutumikila Yehova . Kodi n’kuthekadi kuti maganizo ali m’Baibo ni a Mulungu , osati a anthu ? — 1 Atesalonika 2 : 13 . pangano la mu Edeni . Yesu sanangouza ophunzila ake kuti azilalikila , koma anawauzanso zifukwa zake anafunika kucita zimenezo . Nanga n’ciani cingakuthandizeni kuonjezela cangu canu mu utumiki wacikristu umenewu ? Ndiyeno , Inoki anapeza malo obisalapo ndipo anapumula kwa kanthawi , koma anadziŵa kuti adaniwo amupezabe . Mabanja amapindula kuphunzila nkhani zimenezi pa Kulambila kwao kwa Pabanja . Kenako , wopelekela cikho uja anakumbukila Yosefe . Ambili sadziŵa zimene zimacitika munthu akatsala pafupi kumwalila , ndipo ni ocepa cabe amene anaonapo munthu akumwalila . ( Yohane 3 : 16 ) Citsanzo ca Abulahamu cimatithandiza kuyamikila kwambili dipo , limene ndi njila yaikulu imene Mulungu anatisonyezela cikondi . Ngati muthandiza ena pa mavuto awo , mudzakhala acimwemwe , opanda nkhawa kwambili , ndiponso simudzakhala osungulumwa . ( Miy . 3 : 21 , 23 ) Conco , kudziŵa kuti “ nzelu zopindulitsa ” n’ciani ndi mmene tingaziseŵenzetsele , kudzatiteteza . Sitiwamvela mpaka kufika pophwanya malamulo a Mulungu kapena kutengako mbali pa nkhani za ndale . — Ŵelengani 1 Petulo . Kuganizila mfundo zimene takambilana kungakuthandizeni kwambili kupeleka mphatso zimene zingakondweletse ena . Inafotokozanso kuti Yesu adzaweluza anthu panthawi ya cisautso cacikulu pamene iye “ adzafika mu ulemelelo wake . ” * ZA M’NKHOKWE YATHU Njila ina imene tingasonyezele kuti timaona moyo mmene Yehova amauonela ni mwa kupewa ngozi . Pamene iye anaukitsa mwana wamwamuna wa mkazi wa masiye , mai ameneyu ayenela kuti anadabwa kwambili . Cifukwa cotsatila mfundo zimenezi , Akhristu ofikapo mwauzimu sakhala na mfuti yodzitetezela kwa anthu ena . Onani “ Mafunso Ochokera kwa Owerenga ” mu Nsanja ya Olonda ya September 15 , 2006 , peji 30 . “ Ndinu woyenela , inu Yehova Mulungu wathu wamphamvu , kulandila ulemelelo ndi ulemu , cifukwa munalenga zinthu zonse . ” — CHIV . Uthenga wabwino umenewu umapeleka cenjezo kwa anthu ocita zoipa , komanso ciyembekezo kwa anthu olungama , kuŵatsimikizila kuti madalitso amene ayembekezela adzafika posacedwa . Anthu amenewo amaona kuti ndi kupanda nzelu kukhulupilila kuti kuli mizimu yoipa . 1 , 2 . ( a ) Ndi mphatso zotani zimene Mulungu anapatsa Adamu ? M’nthawi ya atumwi , anthu ambili mu Ufumu wa Roma anali kulankhula Cigiliki . Iye satelo ngati tilapa ndi kum’pempha mwacikhulupililo ndi modzicepetsa kuti atikhululukile pa maziko a nsembe ya dipo la Yesu . ( Sal . Iye anakamba za ‘ Yesu Khristu Mnazareti uja , amene iwo anamupacika pamtengo , koma amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa . ’ Victor , woyang’anila dela wa mu Africa muno anati : “ Ndimayamikila kwambili Yehova kuti ine ndi mkazi wanga sitikhala ndi nkhawa yadzaoneni yakuti cakudya ticipeza kuti komanso sitidela nkhawa kuti tipeza bwanji ndalama zolipila nyumba ya lendi . Ndiyeno , Luka analemba zimene zinacitika pamene Mariya ndi a m’banja lake anapita ku kacisi , apo n’kuti Yesu ali na zaka 12 . Ndiyeno sankhani mmene mudzagwilitsila nchito umoyo wanu . Ngati mufuna kudziŵa zambili , dinizani pa linki yakuti “ Citani Copeleka ku Nchito Yathu ya Padziko Lonse ” pansi pa peji yoyamba pa jw.org , kapena mungalembe kalata ku ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova ya m’dziko lanu . Conco , anayamba kusakila cibowo kunja kwa holoyo kuti amveleko zimene zinali kucitika m’katimo . Posakila - sakila , anapeza malo abwino okwelela , ndipo anakwela holoyo mpaka kufika ku mtenje , pamwamba potalika mamita 4.8 kucoka pansi . Pa nkhani ya kuphunzila Baibulo anthu ena amanena kuti : “ Ndine wotangwanika . ” Baibo imati : “ Sonyezani kuti ndinu oyamikila . ” Baibulo limangokamba kuti Yesu anatengedwa kupita ku Yerusalemu . Popeza malamulo amasiyana malinga ndi dziko , muyenela kufunsanso anthu odziŵa bwino za malamulo ndi misonkho . Kunyumba ya masisitele , tinali kugwila nchito yoyeletsa . ( Mat . 5 : 3 ) Anthu amene amalandila uthenga wathu , timawathandiza kuzindikila zosoŵa zao mwa kuwauza “ uthenga wabwino wa Mulungu . ” ( Ekisodo 21 : 23 , 24 ) Mfundo imeneyi inali kuthandiza oweluza kupeleka cilango coyenelela . M’pake kuti Baibulo limafotokoza kuti Mulungu ndi “ amene mwanzelu zake anakhazikitsa dziko limene anthu amakhalamo . ” Ndithudi , kuphunzitsa ana anu mwa kuuzimu pa Kulambila kwa Pabanja ndi njila imodzi yofunika imene mungakhalile m’busa wabwino . N’napitiliza kupita patsogolo , ndipo m’caka ca 1991 , n’nabatizidwa n’kukhala wa Mboni za Yehova . Ndipo nthawi zonse ndimasangalala kuti zikhulupililo zanu zimacokela m’Baibulo . Tidzaphunzila mmene kupandukila Mulungu m’Edeni kwakhudzila amuna ndi akazi . Zaka 3,000 zapitazo , wolemba ndakatulo wina anati : “ Munandipanga modabwitsa ndipo zimenezi zimandicititsa mantha . ” Cifukwa ca zimenezo , ndinaphunzila kudalila Yehova . ” Nchito yao yolalikila ndi kupanga ophunzila inatsegula mwai wakuti anthu a mitima yabwino akhalenso pamtendele ndi Yehova , akhale naye paubwezi ndi kuti mtsogolo akakhale ana ake auzimu . N’zinthu ziti zimene zinasinthiwa m’buku la nyimbo latsopano ? Nanga mungacite ciani kuti mupindule poliseŵenzetsa ? Kopeyo inakambanso kuti oweluza anali kugamula ndalama zimene wolakwayo anayenela kulipila mwinimunda cifukwa ca zinthu zimene wawononga . Yehova waonetsanso kuti ulamulilo wake wokha ndiwo wabwino mwa kulola zoipa kupitilizabe kwa kanthawi . ( Sal . 147 : 2 ) Wamasalimoyu ataona kuti anthu a Mulungu abwelela ku malo awo olambilila , analimbikitsidwa kutamanda Yehova . Sanafunenso kugwilizana na cipembedzo conama m’njila iliyonse . M’malomwake anaikamo dzina lakuti “ Ambuye . ” Mwacitsanzo , Franz ndi Margit , amene akutumikila ku nthambi ina , anatumikilako ku nthambi ya ku Brazil mu 1982 . Conco , tifunika kupempha Yehova kuti atilanditse kwa woipayo . — Chiv . Sikutanthauza nkhanza kapena kuzunza . — Miyambo 4 : 1 , 2 . ( Mal . 3 : 18 ) Pakali pano , n’zolimbikitsa kudziŵa kuti “ maso a Yehova ali pa olungama , ndipo makutu ake amamva pembedzelo lao . ” — 1 Pet . Ndaona mmene Yehova amasamalila munthu aliyense payekha , kumulandila , kumuthandiza ndi kumudalitsa . Zimenezi zikuphatikizapo kupewa kuyang’ana zithunzi zodzutsa cilakolako , kaya ndi pa kompyuta , pa zikwangwani , pa magazini , kapena pena paliponse . Izi zingakhudze mpingo wonse , maka - maka ngati akulu sakonda kuimbako nyimbo , kapena ngati ali na cizoloŵezi cocita zinthu zina pamene mpingo ukuimba . — Sal . N’zosadabwitsa kuti mwamuna wake , Isaki , “ anam’konda kwambili , ndipo anatonthozedwa pambuyo pa imfa ya mai ake . ” ( Gen . Pa Salimo 34 : 13 , Davide anacenjeza kuti : “ Tetezani lilime lanu ku zinthu zoipa . ” Potsatila citsanzo ca Atate wake , Yesu anagaŵila nchito yofunika kwa ophunzila ake . Ngati tipempha nzelu na mphamvu kwa Yehova tili na cikhulupililo , iye adzatipatsa zimenezi mooloŵa manja . — Yak . Mofanana ndi atumiki ena a Mulungu , nayenso anali kuganizila nthawi pamene Yehova adzamasula anthu ku imfa . ( Yobu 14 : 14 , 15 ; Aheb . Ponena za io , Yesu anati : “ Ndinu odala cifukwa maso anu amaona , komanso makutu anu amamva . ” ( Deut . 32 : 4 ) Mulungu sadzazengeleza powononga dzikoli , ndipo palibe amene adzakayikila kuti ciŵeluzo cimene capelekedwa n’colungama . Ndani Anapanga Mulungu ? — September - October Tikamvela malangizo amenewa , iye amaticitila cifundo . Iwo anayenda makilomita ambili kupita m’miseu ya Aroma , ndipo anadutsa m’malo okwela mumzinda wa Fulugiya , ndi kuloŵela cakumpoto kenako kumadzulo . Tidzakambilananso mmene tiyenela kucitila tikalandila malangizo a gulu la Yehova . ( 1 Akor . Cizindikilo ca kukhalapo kwake cakhala cikuonekela kuyambila mu 1914 . ( Ŵelengani Aheberi 4 : 12 . ) ( Miy . 2 : 10 - 12 ) Mwa ici , timakhalabe m’cikondi ca Mulungu , tili na ciyembekezo ‘ cokalandila moyo wosatha . ’ — Yuda 21 . Abale na alongo onse otumikila pa Beteli ku Brooklyn anauzidwa kuti azisonkhana m’mipingo ya mumzinda wa New York . Kuganizilapo mozama kumeneku kwapangitsa ena amene anali kukhulupilila cisanduliko kusintha maganizo awo . Adilesi ya ofesi ya nthambi iliyonse imapezeka pa webusaiti ya www.jw.org . M’nkhani yoyamba , tidzakambilana mfundo zofunika zimene tingaphunzile pa zitsanzo za anthu ochulidwa m’Baibo awa : Kaini , Solomo , Mose na Aroni . Nthawi imeneyo tinali tisanadziŵane . Tingapindule bwanji ndi mafanizo aŵiliwa ? ( Mat . ( Yoh . 15 : 19 ) Conco , n’napita kukapempha akulu - akulu a bungwelo kuti anipatse mwayi wodziŵika monga mtumiki wa Mulungu . ( Yeremiya 10 : 23 ) Zimene zakhala zikucitika m’mbili ya anthu zaonetsa kuti mau amenewa ndi oona . Nanga ningawathandize bwanji ? Mafunso otsatilawa adzakuthandizani kuona ngati ndinu wokonzeka kubatizidwa : ( 1 ) Kodi ndine wokhwima mwakuuzimu moti ndingabatizidwe ? Komanso mneneli Danieli , amene anakhalapo panthawi imodzi ndi Ezekieli , anakamba mau awa ponena za mfumu ya kumpoto : “ Kotulukila dzuŵa ndi kumpoto kudzacokela mauthenga amene adzaisokoneza . Yendani mmenemu anthu inu . ’ Yendani m’njila imeneyi kuti musasocele n’kuloŵela kudzanja lamanja kapena lamanzele . ” ( Yes . Imfa ndi mdani woopsa kwambili . 8 : 26 ; 14 : 31 ; 16 : 8 ; 17 : 20 ) Anafunika kukhala ndi cikhulupililo colimba ndi kudalila Yehova . Malinga ndi kuona kwa munthu , kodi Mose anali munthu wotani pomuyelekezela ndi Farao ? Zingakhale zovuta kukambitsilana ndi makolo za kusintha zinthu zina panyumba yao kapena zakuti panthawi ina angafunike kusamuka . Cifukwa cakuti tonse timalalikila , timatha kulengeza uthenga wabwino kwa anthu ambili . Kodi Yesu anacoka bwanji ku cipululu kupita ku kacisi ku Yerusalemu ? Rehobowamu anali mwana wa mfumu Solomo , imene inalamulila mu Isiraeli kwa zaka 40 . ( 1 Maf . ndiponso m’zofalitsa zimene zinatulutsidwa posacedwapa pamsonkhano wacigawo . N’cifukwa cake Baibo imakamba kuti anthu oloŵa m’banja nthawi zina “ adzakhala ndi nsautso m’thupi mwawo . ” ( 1 Akor . Cinanso , kusintha kwa zandale , kwacititsa kuti pakhale kusintha kwa zinenelo zokambiwa na anthu ambili . Amayi anali Mboni yokhulupilika . Iye sanapusitsidwe ndi malonjezo a Satana ndipo sanayambe waganizila ubwino ndi kuipa kwa malonjezowo . Ganizani cabe , iwo anaona mankhaka , mavwembe , adyo , na anyezi kukhala zofunika ngako kuposa ufulu umene anapeza wolambila Mulungu woona , Yehova . Katatu konse , ine na mkazi wanga tinapatukana ndipo cikwati cathu cinatsala pang’ono kutha . ” Koma popeza kuti tsopano ndaulula , ndimamva ngati kuti ndatula cikatundu colema . Ndiponso , mofanana ndi milungu yacikanani imene anali kulambila , io anakhala anthu ankhanza , anayamba kupeleka ana ao nsembe ndipo anali kupondeleza osauka . Petulo anali katswili pa kusambila . Akanafuna akanasambila ndi kubwelela ku bwato . Kuti mupeze nkhanizi , pitani pa ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA . “ Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu , ndipo ndi opindulitsa . ” — 2 Timoteyo 3 : 16 . Tiyeni tione mmene Mau a Mulungu angatithandizile kuthetsa mavuto amenewo . Usiku wakuti maŵa adzaphedwa , Yesu anauza mtumwi Petulo kuti : “ Simoni , Simoni ! MOSE anadziŵa kuti akanakhala ndi tsogolo labwino m’dziko la Iguputo . 11 : 35 ) Pambuyo pa kukhadzikitsidwa kwa Ufumu mu 1914 , odzozedwa okhulupilika onse amene anali m’manda anaukitsidwa ku moyo wauzimu kumwamba kuti akathandizane na Yesu kulamulila anthu padziko . — Chiv . Koma ngakhale kuti m’nyimboyo mulibe maina , n’zotheka kudziŵa amene akukamba mwakumva zimene akulankhula . Yesu akaona anthu akuvutika , anali kuwathandiza mwacikondi . Ndi mfundo za m’Baibulo ziti zimene zimatilimbikitsa kusamalila Nyumba zathu za Ufumu ? Kodi ophunzila a Yesu akanapindula bwanji pocita nchito ya Yehova ? Kusamalila banja kunamuthandiza kukhala wacikondi kwambili monga tate . Kunena zoona , n’zosangalatsa kwambili kukhala wanchito mnzake wa Mulungu . — 1 Akor . 21 : 3 ) Citsanzo cake n’cothandiza kwa ife cifukwa cakuti aliyense wa ife angazunzidwe cifukwa ca kukhala wokhulupilika . Ndipo maseŵelo amenewa anali kuonetsedwa mobwelezabweleza . Akhiristu ena akale ‘ anatenga kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . . . kukhala cifukwa cocitila khalidwe lotayilila . ’ Unali wolemela ngako , ndipo anthu a mu mzindawo anali na mtima wokonda zinthu zapamwamba , zosangulutsa , ndi umoyo wa wofu - wofu . ( Sal . 147 : 11 ) Conco , tifunika kukhala na cidalilo cakuti cifukwa ca kukoma mtima kwake kosatha , iye sadzatitaya ndipo adzatithandiza kugonjetsa zilakolako zoipa . Yehova salitenga mopepuka lonjezo limeneli , ndipo aliyense amene wapanga lonjezoli sayenela kuliona mopepuka . ( Mlal . N’cifukwa ciani kukhala maso mwauzimu n’kofunika kwambili masiku ano ? Posacedwapa , akulu ena amene akwanitsa kuthandiza abale kupita patsogolo mwa kuuzimu anafunsidwa kuti afotokoze zimene amacita pophunzitsa ena . M’mbuyomu , takambapo zoonetsa zimenezi . Inde . Mwacitsanzo , Alex * anamangidwa m’ndende ya ku Brazil kwa zaka 19 kaamba ka nkhanza . “ Ndidzalengeza dzina la Yehova . . . , Mulungu wokhulupilika , amene sacita cosalungama . ” — DEUT . Munthu winanso dzina lake Haruichi ndi mkazi wake Tane Yamada , pamodzi ndi acibale ao ambili , analandila coonadi caka ca 1930 cisanafike . Zimene zinacitikila banja lina m’nthawi ya atumwi zingathandize makolo kudziŵa kuculuka kwa cidziŵitso cimene munthu amafunikila kuti abatizike . ( Mac . 3 : 1 - 5 ) Conco , tiyenela kupewa kuwacititsa mantha . ( Mac . 13 : 48 ; 16 : 14 ) Silvana , mpainiya amene watumikila kwa zaka pafupi - fupi 30 , anati : “ Nikalibe kufika pa nyumba ya munthu m’gawo langa , nimapemphela kwa Yehova kuti anithandize kukhala na maganizo oyenelela . ” Pamene ndinali ndi zaka pafupifupi 20 , ine ndi abale anga tinali kucita zinthu zambili zaciwawa . Koma a Willie ananenanso kuti : “ Kodi mungadabwe ngati nakuuzani kuti Yesu atamwalila anapita ku helo ? ” Iye anamangila guwa la nsembe mulungu wamkazi wochedwa Asitoreti ndi guwa lina la mulungu wochedwa Kemosi . Abale na alongo mumpingo anatithandiza ngako . Nanga cipezeka kuti ? Koma ataganiza zakuti nayenso apite , anavutika kupanga cosankha cakuti apite kapena ai . Kodi amuna apaudindo angaphunzile ciani kwa Timoteyo ? Musalole kuti zophophonya za ena zikupangitseni kuwononga ubwenzi wanu na Yehova . Akaimilitsa mtengo , munthuyo anali kumva ululu kwambili cifukwa thupi lake lonse linali kulelemba pa misomali . Amadalitsa Anthu Ofunitsitsa Kupeleka , 12 / 15 ( Chivumbulutso 1 : 20 – 2 : 1 ) N’zoonekelatu kuti Yehova ndi Yesu amakhala nafe pamisonkhano ndipo amatilimbikitsa . Mwamuna wake Vladimir , ndi ana awo atatu aamuna , onse ni akulu mumpingo . N’kutheka kuti m’masomphenyawo , iye anaona dziko losiyana kwambili na limene anali kukhalamo . N’ciani cingatithandize kuti tisakhale ndi mantha na zimene zidzacitika m’tsogolo ? Mwacitsanzo , vuto singasile , ndipo anthu ena osalakwa angaimbidwe mlandu . Ndipo milalang’amba yambili ili m’magulu akuluakulu . — Chronicle . Patapita caka cimodzi , mwana wathu wamkazi , Irina , anabadwa . N’nakondwela ngako , koma cimwemwe canga sicinakhalitse . Kuwonjezela pamenepo , amavala zovala zomenyela nkhondo . Rudolf , amene tinali kuitana kuti Rudi , anandipatsa Baibulo . Mosakayikila , abale na alongo a m’kaguluko anakondwela ngako pamene ofalitsa ena 6 ocokela ku Germany ndi ku Netherlands anasamukila kudela limeneli mu 2015 , kuti akatumikile pamodzi ndi ofalitsa a kudelali . Popeza tikukhala m’masiku otsiliza komanso ovuta , nafenso timakumana na mavuto aakulu . Paulo anakumana ndi cizunzo coopsa , ndipo nthawi zonse anali kudela nkhawa abale . Kutsatila citsanzo ca Timoteyo kungakuthandizeni . Mwacitsanzo , tinasangalala kukhala ndi kamvedwe katsopano ponena za “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu , ” mogwilizana ndi nkhani imene inafalitsidwa mu Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 . Ndithudi tikukhala m’nthawi imeneyi . Mmodzi wa anthu amenewa ndi Yohane M’batizi . Woyang’anila delayo anamuuza kuti : “ Sizinacitike mwangozi kuti nibwele kuno . wamalonda woyendayenda ndi la cuma cobisika ? Matthew anati : “ Ku mpingo umene ndinapitako tinasonkhana 200 koma misonkhano yonse inatsogozedwa ndi mkulu mmodzi wa cikulile ndi mtumiki wothandiza mmodzi wacinyamata . Conco , kamasulidwe katsopano ka Salimo 144 sikanasinthe kamvedwe kathu ka ziphunzitso za m’Baibo . 10 : 16 ) Kukamba zoona , tiyenela kumuyamikila kwambili Yehova cifukwa cotipatsa mwayi wokhala naye paubwenzi wapadela . ( Genesis 4 : 11 - 13 ) Panthawi ina , Yehova anazindikila kuti Baruki wayamba kulefuka ndi kutopa cifukwa ca maganizo olakwika . ( Machitidwe 27 : 9 - 12 ) N’cifukwa ciani anapeleka malangizowo ? Iye anali kufunika kuthandizidwa kuti akhale pa njinga ya olemala , kukhala m’galimoto ndiponso mu Nyumba ya Ufumu . 11 : 9 ) Popeza kuti nyama sizingaphunzile za Yehova , mwauzimu ulosiwu ukukwanilitsika pakati pa anthu . Ndipo zioneka kuti caka na caka ana pafupi - fupi 3 miliyoni amafa cifukwa ca njala . Mau a Mulungu , amene ni cida cathu cofunika kwambili pophunzitsa , angatithandize polangiza ena m’cilungamo . Popeza kuti tikali m’dziko loipa , nthawi iliyonse tingacitilidwe zinthu zopanda cilungamo . Ngati mukufuna kubatizidwa , kodi mungakonzekele bwanji ? Kufika panthawi ino , ine ndi mkazi wanga tathandiza anthu 80 kukhala a Mboni za Yehova mwa kuphunzila nao Baibulo . Ngakhale kuti maina ao sanalembedwe pa zinthu zimene anapanga , ayenela kuti anakhutila podziŵa kuti Mulungu wadalitsa nchitoyo . ( Miy . Tsiku la cikwati cathu Mkhiristu aliyense angayambe kulabadila thupi lake locimwa . * Kuyambila mu 1944 , ndeke zambili za nkhondo zinagwetsa mabomba mumzinda wa Kent . Kuti atengeko mbali panchito yofunika yolalikila imeneyi , ena afeŵetsa umoyo wao , aphunzila cinenelo ndi cikhalidwe cina . Kunena zoona , iwo anacita zonse zimene Yesu anauza otsatila ake kucita . — Mac . 1 : 8 ; Akol . Pali zitsanzo zambili zimene zimaonetsa kuti Mulungu wakhala akucilikiza gulu lake ndipo zimenezi zionetsa kuti iye “ si Mulungu wacisokonezo , koma wamtendele . ” — Ŵelengani 1 Akorinto 14 : 33 , 40 . MULUNGU ANAKHAZIKITSA ATUMIKI AKE M’NTHAWI ZAKALE Kodi Rehobowamu atamvela Mulungu , zotulukapo zake zinali zotani ? Kodi pafunika kukhala kusiyana kotani pakati pa anthu amene amatumikila Yehova na amene sam’tumikila ? Mulungu anadalitsa anthu aŵili oyambilila ndi kuwapatsa nchito yosangalatsa kwambili . ( b ) N’ciani cimene cingasokoneze mgwilizano pakati pa Akhristu ? Thorn , amene anali woyang’anila woyendela kuyambila mu 1894 . Yesu anali kum’konda Marita cifukwa cakuti anali wokoma mtima , woceleza , ndi wolimbikila nchito . Izi n’zimene anacita Zedekiya , mfumu yothela kukhala pa mpando wacifumu ku Yerusalemu . Kupitila m’dipo limene anapeleka , Yehova adzathandiza ana ake onse kukhala olungama kothelatu . Ndi cinenelo citi cimene Yesu anali kukamba pophunzitsa ophunzila ake ? Koma buku locedwa Jehovah la mu 1934 , linakamba kuti Cikumbutso siciyenela kucitidwa ndi “ mitima yacisoni ” cifukwa coganizila imfa yowawa ya Yesu , koma ciyenela kucitidwa ndi “ mitima yacisangalalo ” podziŵa kuti iye akulamulila kuyambila mu 1914 . Zimene anacitazo zinali cizindikilo cakuti akulemekeza munthu amene anali kudzakhala mwamuna wake . Iye anakamba kuti : “ Kuphunzila za Yehova m’citundu cimene n’naphunzila kusukulu kunanithandiza kupita patsogolo . ” 2 : 17 ; 1 Yoh . 3 : 13 . Komabe , Yehova yekha ndiye ali na udindo wodziŵitsa anthu cabwino na coipa , ndipo “ mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa , ” umene unali m’munda wa Edeni , unali kuimila udindo wake umenewu . N’ciani cimene mtundu watsopano wa anthu unali kudzacita pokhala “ anthu odziŵika ndi dzina [ la Yehova ] ” ? Ngati pabuka mikangano , kodi timacita bwanji ? ( Mac . 7 : 22 ) Ganizilani mwai umene Mose akanakhala nao . Ukwati umenewu ndi cocitika cosangalatsa kwambili cochulidwa m’buku la Chivumbulutso . ( Chiv . Yehova Mulungu anakonza njila yothetsela mavuto amene amabwela kaamba ka ucimo ndi kutimasula kucilango ca imfa yosatha . Koma Husai anakhalabe wokhulupilika ndipo anali wokonzeka kuika moyo wake paciopsezo kuti alepheletse ciŵembu cimene Abisalomu anakonza . Ndiye cifukwa cake ngakhale pambuyo pa zaka zambili , Aroni ndi ana ake anaonedwabe kuti anali okhulupilika kwa Yehova . — Sal . 14 : 31 ) Yesu ananenanso kuti : “ Atatewo amakonda Mwana wake . ” Daniel anati : “ Tikalibe kucoka ku Spain , sitinali kudziŵa kuti tidzakwanitsa kukhala na umoyo wosalila zambili . Mwacitsanzo , lemba la Ezekieli 14 : 13 , 14 limati : “ Ngati dziko landicimwila pocita zosakhulupilika , ndidzalitambasulila dzanja langa n’kuthyola ndodo zake zimene amakolowekapo mikate yoboola pakati . N’nali kukhulupilila kuti kulibe Mulungu . 115 : 16 ) Iye amatipatsanso cakudya ndi zinthu zina kuti tikhalebe ndi moyo . ( Mateyu 8 : 14 ; Maliko 1 : 29 - 31 ; 1 Akorinto 9 : 5 ) Cifukwa ca makhalidwe a ciwele - wele amene anawanda m’dziko la Roma , Paulo analemba kuti ngati woyang’anila wacikhristu anali wokwatila , anafunika kukhala “ mwamuna wa mkazi mmodzi , ” ndiponso wa ana omumvela . — 1 Timoteyo 3 : 2 , 4 . Kodi timalephela kukhala wololela , kapena timadziwika kuti ndise anthu “ odzetsa mtendele ” ? — Yak . Ningapeŵe bwanji kuloŵelela kwambili m’zamalonda m’dzikoli ? Koma a m’banja langa , makamaka mng’ono wanga Araceli , anali kukamba kuti ndinali kukhulupilila zinthu zabodza . Mulungu wathu wacilungamo nthawi zonse amacita zinthu zoyenela , ndipo ise timafuna kutengela citsanzo cake . 10 : 33 . Cifukwa cokhulupilila kwambili Yehova Mulungu ndi Mwana wake , Yesu Kristu , io adzamvela lamulo la Yesu lakuti : “ Zinthu izi zikadzayamba kucitika , mudzaimilile cilili ndi kutukula mitu yanu , cifukwa cipulumutso canu cikuyandikila . ” Nkhaniyo imatiuza kuti kumeneko “ anali kulimbitsa mitima ya ophunzila ndi kuwalimbikitsa kuti akhalebe m’cikhulupililo . ” 41 : 39 - 41 ; 42 : 6 ) Mbadwa za Yakobo zinaculuka kwambili ndi kukhala “ mitundu yambili ya anthu . ” — Gen . 48 : 4 ; ŵelengani Machitidwe 7 : 17 . ANTHU ambili ali na maganizo osiyana - siyana pankhani ya moyo na imfa . 3 : 6 ) Ganizilaninso Rabeka , amene anali mphatso yocokela kwa Yehova ndipo anakhala mkazi wabwino . Nthawi yogwila nchito monga wopeleka cakudya mu hotelo inapita kale . Ngakhale kuti kapolo aliyense analandila ciŵelengelo ca matalente cosiyana , kodi mbuye wao anali kufuna ciani ? 44 : 22 ; 1 Pet . Pofika mu 2014 , Baibulo limeneli kapena mbali yake linasindikizidwa m’zinenelo 128 , kuphatikizapo zinenelo zina zimene zimakambidwa ku South Pacific . “ Baibulo ndi lovuta kulimvetsa ” . Ndipo akadzaukitsidwa m’dziko latsopano , Bezaleli ndi Oholiabu adzasangalala kwambili kudziŵa kuti cihema cinagwilitsidwa nchito pa kulambila koona kwa zaka 500 . Tifunitsitsa kudziŵa kuti ni liti pamene anthu a Mulungu anamasukilatu mu ukapolo wa m’Babulo . Anthu amene amalambila Mulungu ali na cifukwa cina cokanila kukhulupilila zakuthambo na kuwombeza . N’cifukwa cake anatiphunzitsa kupempha kuti : “ Mutilanditse kwa woipayo . ” Anthu ambili amene timawaitanila ku Cikumbutso amaisunga pamtima lemba limeneli . Pa zitsanzo zimene takambilana , ca Adamu , Hava , na angelo opanduka , tiphunzilapo mfundo ziŵili zofunika kwambili . * ( 1 Yohane 4 : 9 , 10 ) Popeza Yehova Mulungu ndiye gwelo la kupatsa , ndipo tinapangidwa m’cifanizilo cake , si zodabwitsa kuti tikatengela khalidwe lake la kupatsa , tidzapindula , ndipo iye adzatiyanja . — Aheberi 13 : 16 . 3 Zimene anaŵelengazo zinamulimbikitsa kuti ayambe kuphunzila Baibo na Mboni za Yehova . Koma zinam’tengela nthawi yaitali kuti athetse cizoloŵezi cake coipa . ( b ) Kodi Akristu ayenela kudziŵa ciani pankhani yothetsa mikangano ? Zimenezo zinandicititsa cidwi kwambili . Tingatengele phunzilo pa cocitika cotsatilaci : Mlongo wina atafika kuphwando , anapatsa moni abale aŵili . Kwa zaka zambili , ndinaona kuti anthu amene anali kupita ku chalichi nthawi zonse , sanali kucita zimene Yesu anaphunzitsa . Cifukwa cakuti Yehova akuthandiza Mboni zake , ciŵelengelo cao cikukula kwambili . Mu 1965 , ndisanakwatile , anandiitana kukaloŵa Sukulu ya Gileadi ya nambala 41 . 15 : 3 , 4 ; 21 : 5 . Conco , panafunika kufewetsa mau ena . Pamsonkhano wapacaka wa nambala 129 wa Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania , umene unacitika pa October 5 ndi 6 , 2013 , panapezeka anthu 1,413,676 ocokela m’maiko 31 . Ena anaonelela pulogalamuyi kudzela pa intaneti . Mofanana ndi kholo lake Abulahamu , Mose anali ndi cikhulupililo cakuti Yehova adzaukitsa akufa . Ubatizo wathu umaonetsa kuti “ ndife a Yehova . ” amayamikila ndi kudalitsa anthu amene amam’tumikila mokhulupilika ? Gawo la padziko lapansi la gulu la Yehova likukula m’mbali zosiyana - siyana . Koma kukula kumeneku kumaitananso masinthidwe . Zimenezi zimatikumbutsa za abale na alongo athu a m’zaka 100 zoyambilila , amene anali na ciyembekezo copita kumwamba . Anthu oposa 8 miliyoni a Mboni za Yehova , ocokela m’maiko oposa 240 , apeza njila yabwino yothetsela nkhanza . Kodi kuphunzila kuti tiziganiza monga Khristu kungatithandize bwanji ? Pamisonkhanoyo n’naona abale na alongo anga ambili - mbili . Masiku ano , m’malo mokhala ndi mtumiki wa mpingo ndi wothandiza mtumiki wa mpingo , pa bungwe la akulu lililonse pamaikidwa mgwilizanitsi ndi kalembela . Iwo anati : “ Tinali kuphunzila ndi anthu 15 kapena kuposa pamenepo , koma tinacepetsako maphunzilo a Baibulo . Tinali kucititsa maphunzilo 10 cabe . ( Mateyu 22 : 39 ) Ngati mumapindula ndi uthenga umenewu , ndi umboni wakuti Yehova amakukondani . M’malo mokhumudwa , iye apitilizabe kupilila , ndipo anakhalabe wokhulupilika panthawi yovutayi . — Yakobo 1 : 4 . ‘ Muzikwanilitsa Zimene Mwalonjeza , ’ Apr . Popeza Yehova amadyetsa ngakhale makwangwala , mufunika kukhala na cikhulupililo cakuti adzakupatsani zofunikila pa moyo wanu . — Sal . Mulungu anafunsa Kaini kuti : “ Kodi iweyo suugonjetsa ? ” Zimene tingaone pa malo amenewo zingatipangitse kukhala ndi zilakolako zoipa , ndipo pamapeto pake tingacimwile Yehova . Coyamba , Paulo anakamba kuti anapitiliza kulalikila kwa Ayuda cifukwa anali ‘ kufunitsitsa mumtima mwake ’ kucita zimenezo . Kodi pali zifukwa zabwino zofotokozela nkhani za m’Baibulo mwa njila imeneyi ? M’caka ca 1914 , nkhondo inabuka pakati pa maiko a ku Ulaya ndipo inafalikila pa dziko lonse lapansi . Ngati ndimwe kholo kapena mkulu , ndipo mufuna kupeleka cilango kwa mwana kapena kwa Mkhristu mnzanu , muyenela kutengela citsanzo ca Yehova . Muyenela kuzonda coipa cimene munthuyo anacita kwinaku mukuyesetsa kuyang’ana zabwino mwa iye . — Yuda 22 , 23 . Tsiku lina pamene tinali kuphunzila , msilikali wina wolondela ndendeyo anatipeza ndipo anatilanda mabuku . 5 : 3 ) Iwo amakopeka kwambili ndi zinthu za m’dzikoli zimene zimacititsa kuti akhale ndi ‘ cilakolako ca thupi ndi cilakolako ca maso . ’ ( 1 Yoh . 2 Anati : “ N’cifukwa ciani wapsa mtima conco , ndipo nkhope yako yagwelanji ? Ngati tili na cisoni cacikulu cifukwa cakuti tilibe mwana , kapena cifukwa wokondedwa wathu anamwalila , n’zotheka kupeza citonthozo . Khalani wokonzeka kukambilana na mwana wanu nthawi iliyonse imene wafuna . Koma tsopano ndine wokondwela kwambili . Tiyeni tioneko zitsanzo zina zocepa . Cifukwa cotikonda , Yehova wacititsa kuti Mau ake Baibo , amasulidwe m’zinenelo zambili kuti ‘ anthu kaya akhale a mtundu wotani , adziŵe coonadi molondola . ’ Inde , mofanana ndi wamasalimo , naise tingapemphe Mulungu kuti : “ Ndiphunzitseni kucita zabwino , kulingalila bwino ndi kudziŵa zinthu . ” — Sal . 10 : 16 ; Aroma 5 : 1 , 2 ; Yak . 2 : 21 - 25 ) Ngakhale masiku ano , dipo limatithandiza kukhala pa ubwenzi wabwino ndi Atate wathu , ndi kutengako mbali pa kuyeletsa dzina lake . * Mwina Sara anaganiza kuti zimenezo zidzathandiza kuti colinga ca Mulungu cotulutsa mtundu mwa Abulahamu cikwanilitsidwe . Panthawiyo , anthu ambili adzafuula mwamantha kuti : “ Ndani angaimilile pamaso pao ? ” ( Chiv . Ndipo gulu lanu lili cabe ndi asilikali 580 sauzande , kutanthauza kuti ndinu ocepa kuwilikiza kaŵili poyelekezela ndi adani anu . 19 : 9 ) Koma nthawi ya ukwati isanakwane , pali cinacake cimene cidzacitika . Mungakonze bwanji ndandanda yoŵelenga Baibulo tsiku lililonse ? Kusintha kwa zinthu mu umoyo wathu , kapena mu utumiki wathu , kungakhale ciyeso pa kudzicepetsa kwathu . MATENDA AAKULU NA KULEMALA ZIMASINTHA KWAMBILI UMOYO WA MUNTHU . Sudzabwela Kawalala angathe kubisa colakwa cake kwa akulu - akulu a boma , mabwana ake , akulu , kapena kwa makolo . Mlengi wathu , Yehova , amadana ndi kupanda cilungamo . N’zosavuta kukhala na mzimu wonyada ndi wodzikweza . 16 Kodi Mudzakambilana Kuti Muthetse Mkangano ndi Kulimbikitsa Mtendele ? ( Sal . 94 : 14 ) Iye sangatitaye olo titakumana na mavuto aakulu bwanji . Pamene atumwi anali kutsutsidwa ndi Asaduki , sanaleke kuphunzitsa m’dzina la Yesu . — Mac . 5 : 17 , 18 , 27 - 29 . Pa Yeremiya 31 : 15 pamati : “ Yehova wanena kuti , ‘ Mau amveka ku Rama . Koma tizimvela mocokela pansi pamtima malamulo apamwamba a Yehova , amene ndi “ Woyela , ” ndi kutengako mbali mwakhama pa “ nchito yolengeza uthenga wabwino wa Mulungu . ” Ngakhale kuti ni opanda ungwilo , makolo acikondi amaphunzitsa , kulimbikitsa , kuthandiza , na kupeleka cilango kwa ana awo , cifukwa amafuna kuti akhale na umoyo wacimwemwe komanso waphindu . Mu 1900 , pafupifupi zaka 21 pambuyo poti ayamba kufalitsa magazini a The Watch Tower , m’dzikolo munali cabe magalimoto pafupifupi 8,000 , ndipo miseu yabwino inali yoŵelengeka cabe . Koma ubatizo ni ciyambi cabe . Kodi Mwiitiyopiyayo anacita ciani atamva uthengawo ? Ngakhale kuti Solomo anacokela ku banja lokonda kwambili zinthu zauzimu , ndipo poyamba anali mfumu yabwino , m’kupita kwa nthawi anaononga colowa cake cakuuzimu . M’zaka zonsezi , Angie wakhala wokhulupilika kwambili kwa Yehova . Zimenezi zapangitsa banja lathu kukhala lolimba . 12 : 23 . Pamene mpingo wacikristu unakhazikitsidwa pa Pentekosite mu 33 C.E . , coonadi ndi kuona mtima zinayamba kuonjezeka . 38 : 18 - 23 . Komanso , magazini ya Galamukani ! Kumbukilani kuti mtumwi Petulo anakamba kuti Yesu anatisiyila citsanzo kuti titsatile mapazi ake mosamala kwambili . ( 1 Pet . M’malomwake , “ khalanibe maso . ” Uzim’kumbukila m’njila zako zonse , ndipo iye adzaongola njila zako . ” — Miyambo 3 : 5 , 6 . Mwa kugwilitsila nchito fanizoli , iye anali kuonetsa kuti uthenga wa Ufumu uli ndi mphamvu yofalikila paliponse ndi kusintha anthu . Ni kuseŵenzetsa mfundo za m’Malemba . Inde , ndi Yehova yekha amene akanapulumutsa Paulo . Gwilitsitsani coonadi cimene munaphunzila , ndipo muzikumbukila kumene munaciphunzilila . Hans ndi Brook , amene ali pa banja , ali ndi zaka za m’ma 30 ndipo ndi apainiya . Kudzatithandiza kuti tizikonda kwambili Mau a Mulungu . Baibulo limati : “ Yehova azidzayembekezela kuti akukomeleni mtima ndipo adzanyamuka kuti akucitileni cifundo , pakuti Yehova ndi Mulungu amene amaweluza mwacilungamo . Tili ndi zifukwa zomveka zokhulupilila kuti posacedwapa malonjezo amenewa adzakwanilitsidwa . Koma sikuti tifunika kucita zimenezi mwa mwambo cabe kuti tikapulumuke pa cisautso cacikulu . Kodi muli ndi funso pankhani ina ya m’Baibulo ? Mwacitsanzo , akatswili a zakuthambo sangatiuze bwino - bwino mmene thambo linakhalilako , kapena cifukwa cake tili pa Dziko Lapansi , ndi zamoyo zina zambili - mbili . Ngakhale kuti azibusa awo anakwiya kwambili , Ophunzila Baibo sanabwelele m’mbuyo pa nchito yofunika imeneyo . ( Yes . 49 : 13 ; Mat . 15 : 32 ) Ngati tiphunzila Baibulo , tidzazindikila kuti Yehova amatikonda , ndipo nafenso tidzam’konda kwambili . Koma si zoona kuti Toñi anafika mocedwa ku nchito . Sikuti Khiristu anapeleka dipo cifukwa ca zolengedwa zonse . Kodi amatiphunzitsa ciani za mmene iye amaonela moyo ? Ana anu akamakumvelani mukupempha Yehova kuti akuthandizeni , amaphunzila kuti naonso afunika kudalila Yehova ( a ) Tingacite bwanji kuti tizipindula ndi kulambila kwa pabanja ndi phunzilo laumwini ? Mwacitsanzo , m’Malemba Aciheberi , timapezamo mau akuti : “ Zolinga za munthu wakhama zimam’pindulila , ” ndi akuti : “ Ciliconse cimene dzanja lako lapeza kuti licite , ucicite ndi mphamvu zako zonse . ” Ŵelengani 1 Timoteyo 3 : 1 . 10 : 16 ) N’zosangalatsa kwambili kuphunzila mfundo za coonadi zimenezi komanso kuziphunzitsa kwa atsopano . ( Miy . 3 : 5 - 7 ) Labadilani pempho lake lacikondi lakuti : “ Mwana wanga , khala wanzelu ndi kukondweletsa mtima wanga . ” ( Miy . Tsiku lina , munthu wina amene anali kudziŵa bwino Cilamulo ca Mose , anafunsa Yesu kuti : “ Kodi lamulo lalikulu kwambili m’Cilamulo ndi liti ? ” ( Salimo 13 : 5 ) Mofanana ndi Davide , masiku ano atumiki a Mulungu ayenela kupitilizabe kupemphela mpaka Mulungu atawapatsa zopempha zao . — Aroma 12 : 12 . N’ciani cimalimbikitsa Akhristu kuthandiza alendo ocokela m’maiko ena ? Nthawi ina izi zisanacitike , Yesu ‘ anamvela cifundo ’ khamu la anthu limene linabwela kwa iye . N’kutheka kuti mwaonapo acicepele ena amene anabatizika , koma pambuyo pake anayamba kukayikila ngati kutsatila mfundo za Mulungu n’cinthudi canzelu . Tsiku lina ndinaima pamzele wogula cakudya popanda kudziŵa kuti cimene cikugulitsidwa n’ciani . UBALE WA PADZIKO LONSE : Cifukwa cakuti timakondana , timadziŵa kuti tikapita ku mpingo uliwonse wa Mboni za Yehova padziko lapansi , abale ndi alongo adzatilandila bwino kwambili . Ndinaganizila cifukwa cake ndifuna kukhala mpainiya , ndipo ndinapemphanso abale ndi alongo okhwima mwa kuuzimu kuti andithandize . Na imwe mungawonjezele mtendele umenewu mwa kuyesetsa kukulitsa khalidwe limeneli , lomwe ndi mbali ya cipatso ca mzimu . Ndinali waukali ndi wankhanza kwa aliyense . Analimbikilabe kucita zinthu mogwilizana ndi mapemphelo awo . Malinga ndi zolemba zimenezo , n’zoonekelatu kuti Mulungu amadalitsa anthu amene amakonda anzao . ( Genesis 41 : 1 - 8 ) Mwina anthuwo anasowelatu conena kapena anali kumasulila zinthu zotsutsana . Mulimonse mmene zinalili , Farao anagwilitsidwa mwala . Kodi abale ndi alongo amenewa ali ndi nkhawa ponena za kumene adzakhala kapena nchito imene adzagwila nchito yomangayo ikadzatha ? Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti anali kukonda anthu ? ( Yobu 4 : 19 ; 25 : 6 ) Mwina tingaganize kuti Elifazi ndi Bilidadi anali kuonetsa kudzicepetsa pokamba mau amenewa . Koma kambili amakhala osiyana . 11 : 8 . Mulungu amatipatsa cilango n’colinga cakuti atiumbe . Conco , tiyeni tipitilize kukhala monga dongo lofewa m’manja mwake . Kodi adzanithandiza kuulimbitsa ? Kodi zofalitsa zathu zikumasulidwa m’zinenelo zingati ? Nanga mapulogalamu a pakompyuta akhala othandiza bwanji pa nchitoyi ? Ndipo panthawi ya nkhondoyo , kodi abale athu ena anataya cikhulupililo cawo ndi kutengako mbali m’za ndale , cakuti Yehova anakhumudwa nawo ? ( Aroma 2 : 20 ) Mwacitsanzo , pa makonzedwe okhala na mizinda yothaŵilako , akulu aphunzilapo mmene angaweluzile milandu mogwilizana na “ cilungamo ceni - ceni . ” kudziŵa malemba oyela . Ophunzila a Yesu anali kudziŵa kuti sakanakwanitsa nchito yolalikila mwa mphamvu zao zokha . Otsalila a Akristu odzozedwa amakonda kwambili anzao amenewa . Iwo amasangalala kudziŵa kuti Atate a Mkwati , Yehova , apatsa mwai anzao amenewa wakuti adzasangalale nao pa cikwati ca Mwanawankhosa cimene cidzacitikila kumwamba . M’Baibulo muli zitsanzo za anthu ambili amene analandila colowa cakuuzimu koma analephela kukhala oyamikila . Sitifunika kukayikila zimenezi . Cioneka kuti amene analemba mau amenewa ndi Davide . Iye ananena kuti : “ Akazi acikulile . . . akhale aphunzitsi a zinthu zabwino . ” — Tito 2 : 3 . Ndipo iyi sinali nthawi yoyamba kuti moyo wa atumiki a Mulungu ukhale pa ngozi mu Iguputo . Kodi tingaphunzile ciani pa zimene zinawacitikila ? Nanga tingapewe bwanji kucita zolakwa ngati zimene iwo anacita ? Khalani ndi colinga cogwila nchitoyo mwaluso ndiponso mwamsanga kwambili . Koma kodi timakwanitsa bwanji kugwila nchito imeneyi ? Yesu anali kumvela cifundo anthu ena . Mwacitsanzo , mphamvu yokoka zinthu kuti zigwe pansi imapangitsa cifungadziko ( atmosphere ) kufungatila dziko lapansi , kukhalitsa bata mafunde a panyanja , komanso kucilikiza zamoyo padziko . Kucokela ali mwana iye anaphunzitsidwa kuzonda anthu a ku dziko la Serbia . Zimenezi zinathandiza ophunzilawo kulalikila popanda zovuta . 19 : 6 . Ngati timatelo , ndiye kuti timaganizila kwambili zimene timafuna . Mungaitane banja lacinyamata kuti lidzapezeke pa kulambila kwanu kwa pabanja . Nanga n’ciani cingatithandize kukhala alendo abwino ? Komanso , zipembedzo zambili zimapangitsa anthu kuona ngati Mulungu ni woipa mwa kuphunzitsa za moto wa helo , kukakamiza anthu kupeleka cakhumi , kapena kucilikiza zandale . 5 : 11 - 14 ) Zotulukapo zake n’zakuti ena akhala na mtima wofunitsitsa kulemela , ndipo sakhutila na zimene ali nazo . Mawu a Mulungu ali ndi mphamvu yotha kuyeletsa munthu . Mofanana ndi Yobu , ena angakambe mosaganiza bwino nthawi zina . Kuti tipeze yankho , tiyeni tikambilane zimene Baibulo limanena zokhudza mapemphelo a anthu a Mulungu . Mwina amaganiza kuti : ‘ Kuphunzitsa ena n’kofunika , koma mumpingo muli maudindo ena ofunika kusamalidwa mwamsanga . Damaris lomba watumikila monga mpainiya kwa zaka 20 . ( b ) N’cifukwa ciani Paulo anamvela mwanjila imeneyo ? ( Deuteronomo 32 : 4 ) Ngati n’conco , kodi zingakhale zomveka kuti Mulungu amene ndi “ wolungama ndi woongoka ” acititse mavuto n’colinga cakuti alange anthu kapena kuwayeletsa ? Tikacita zimenezo , acibale athu angaleke kugwilizana nafe ndipo tingayambe kuona kuti tilibe anzathu . Conco , Atate wathu wakumwamba adzacitapo kanthu kuti atipulumutse . 5 : 8 , 9 ) Pokamba mau a pa 1 Akorinto 10 : 13 , Paulo anayelekezela ndi mayeselo amene Aisiraeli anakumana nawo m’cipululu . N’zoona kuti amabadwa na cikumbumtima , koma cimafunika kuphunzitsidwa . Baibo imeneyi ni yomasulidwa na Mboni za Yehova , ndipo ipezeka m’zitundu zoposa 130 . ( Luka 22 : 52 ) Pamene Petulo anatenga lupanga n’kumenya nalo kapolo wa mkulu wa ansembe , Yesu anam’lamula kuti : “ Bwezela lupanga lako m’cimake . ” Iye anali kudziŵa zambili ponena za Yehova Mulungu wake , ndipo palibe amene akanatha kumulanda zimenezo , kaya kutayikilidwa banja lake , kaya zovuta za paulendo wautali wopita ku Iguputo , ngakhale kucita manyazi pogulitsidwa kwa munthu wacuma wa ku Iguputo dzina lake Potifala . Mnzanga ameneyu ndinali kum’konda kwambili . 17 : 5 ) Palibe cimene cionetsa kuti iye anali kuyembekezela zoposa pamenepa . Cosankha canga cocita upainiya canithandiza kupewa nkhawa imene anthu amakhala nayo pa nchito ndiponso nakhala na mwayi wotumikila Yehova mwacimwemwe kwa zaka zambili . ” Ciwalo cimeneci n’copangiwa mocoloŵana kwambili kuposa cinthu cina ciliconse m’cilengedwe codziŵika kwa anthu . Ngati munthuyo amalemekeza Mau a Mulungu ndipo amafunitsitsa kuphunzila , kukambilana kwa conco kungam’cititse kufuna kuphunzila zambili . — Mac . 17 : 11 . ( 1 Petulo 5 : 7 ) Maka - maka mau a pa Yeremiya 29 : 11 , ananikhudza mtima kwambili . Amasorete anapewelatu kusintha uthenga wa m’Baibulo . ZOCITIKA ZA PADZIKO : Ulosi wochulidwa m’buku la Mateyu caputala 24 ukufotokoza zocitika za padzikoli zimene zinali kudzakhala cizindikilo ca mbali zambili . ( Machitidwe 17 : 27 ) Uphungu wa m’Baibo wakuti tikhale pa ubwenzi na Mulungu ungatithandize kupeza tsogolo labwino . Anthu okhulupilika ochulidwa m’Baibulo anali kuganizila zinthu zimene Mulungu anawalonjeza . Magazini ino ya Nsanja ya Mlonda , ikamba zimene Yesu na Atate wake afotokoza ponena za kumwamba . Anaŵelenga lembali katatu . Ndipo ngati pali dzina limene limachulidwa kwambili m’Baibulo , ndi dzina lake . M’pemphelo limenelo Davide anapitiliza kuti : “ Koma ine ndakhulupilila kukoma mtima kwanu kosatha . ” ( 1 Yohane 1 : 7 ; 5 : 13 ) Nanga dipo lidzapindulitsa bwanji okondeka athu amene anamwalila ? Kodi imwe mukanakhala woloŵa manja mwa njila imeneyi ? A Inoki : Inde , ndi mmene zilili . Ulendo wake unalembedwa m’Baibulo . Timasankha nkhani zosiyanasiyana za m’Baibulo ndi kukambilana malemba ogwilizana ndi zimene tikuphunzila . Monga mmene Baibo inakambila , Yehova akusonkhanitsa “ khamu lalikulu la anthu . . . locokela m’dziko lililonse , fuko lililonse , mtundu uliwonse , ndi cinenelo ciliconse . ” Tiyenelanso kum’konda ndi ‘ moyo wathu wonse , ’ kutanthauza kuti mbali zonse za umoyo wathu ziyenela kuonetsa kuti timam’konda . Harold Corkern M’malo mocita zimene ife tiona kuti n’zoyenela , tiyenela kuganizilapo mozama ndi kusankha zinthu zokondweletsa Yehova . Nchito yosamalila makolo anu okalamba ingakhale yovuta . 1 : 1 , 2 ; Luka 11 : 13 . Ophunzila a Yesu anaona zozizwitsa zimene iye anacita , anamvetsela maulaliki ake , komanso anaona mmene anali kucitila zinthu ndi anthu osiyana - siyana . Koma monga mmene lemba la Mlaliki 7 : 8 limakambila , “ mapeto a cinthu amakhala bwino kuposa ciyambi cake . ” — Felisa . 11 : 1 ) Mwina mungadzifunse kuti , kodi ciyembekezo cingakhale bwanji cotsimikizika ? 15 : 28 ) Nanga tingacite motani zimenezi ? Tingacite zimenezi pamene ndi mtima wonse tigwila nchito ‘ yophunzitsa anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzila . ’ ( Mat . Kodi tifunika kukumbukila ciani pa nkhani ya kutsatila malangizo ? Vuto la Padziko Lonse 3 7 : 10 . Anakana Yehova monga Atate wawo , ndipo anadzikanganula okha ku ulamulilo wake wopeleka citetezo . — Gen . 12 : 1 , 2 ) Kodi mukanacita ciani pamene Aroni ndi Mose analephela kulemekeza Yehova , panthawi imene Iye mozizwitsa anawatulutsila madzi ku Meriba ? — Num . ( b ) Kodi Mulungu amawaona bwanji anthu amene amatsatila mfundo zake ? Mtumwi Paulo anatilimbikitsa kukhala anthu auzimu . Yehova anaona kuti makhalidwe oipa a m’banja la Ahabu anali kufalikila kwa anthu ena . ( b ) Ndi citsanzo citi ca Ayuda cimene Akristu amatsatila ? Tikakhala wocenjela , timasamala kwambili ndipo timakhulupilila nkhani imene ndi yoona . Ngakhale kuti timafuna kukhala ndi thanzi labwino , timaika maganizo athu pa kutumikila Yehova ( Onani ndime 17 ) Kuzindikila cifunilo ca Yehova : Kudziŵa kapena kuzindikila mmene Yehova amaonela zinthu ndi zimene zimam’kondweletsa . Mwacitsanzo , pambuyo pakuti mphepo yamkuntho yaononga mizinda ina m’dziko la Philippines mu November 2013 , meya wa mzinda wina waukulu anati : “ Zioneka kuti Mulungu anali kwinakwake . ” ( Ŵelengani Aefeso 4 : 1 - 6 , 15 , 16 . ) Tingadzipende bwanji kuti tidziŵe ngati timakonda zosangalatsa moyenela ? N’kutheka kuti munapempha thandizo koma ena anakukhumudwitsani cifukwa sanakuthandizeni m’njila imene munali kuyembekezela . Nthawi zina ndinali kuganiza kuti sindinali kufunika kukonda Yehova kuposa makolo anga pa mlingo umenewu . Mwacitsanzo , kuopa Mulungu kumatilimbikitsa kupewa makhalidwe oipa monga ucakolwa ndi ciwelewele . — 1 Akorinto 6 : 9 , 10 . N’kofunika kwambili kuti muziphunzitsa ana anu kuona phindu la mfundo za m’Baibulo . Kuwonjezela pa kupeleka mphatso za ndalama kapena zinthu zina zamtengo wapatali , pali njila zinanso zopelekela zinthu zothandiza pa nchito yolalikila padziko lonse . Imeneyi ndi njila yabwino kwambili yogwilitsila nchito moyo wanga . ” Ndiye cifukwa cake anauzila Petulo kulemba kuti : “ Inu okondedwa , popeza mukudziŵilatu zimenezi , cenjelani kuti musasocele pokopeka ndi zolakwa za anthu ophwanya malamulowo , kuopela kuti mungalephele kukhala olimba ndipo mungagwe . ( 1 Timoteyo 5 : 8 ) Caciŵili , munthu amene amasamalila banja lake mwakhama amathandiza a m’banja lake kuona kuti kugwila nchito mwamphamvu n’kofunika . Kodi simukanayamikila ngati akulandilani bwino ku Nyumba ya Ufumu , ngakhale kuti mwacokela kudziko lina kapena muli na khungu losiyanako ? N’zoona kuti nthawi zina timakhumudwitsana , koma timacita khama kuti tizilemekezana , cifukwa n’zimene timafuna m’banja lathu . ” Muzicita zimenezi nthawi iliyonse , osati cabe pokonzekela misonkhano , kapena pa kulambila kwa pabanja . Pa anthu onse amene anakhalako padziko lapansi , Khristu yekha ndiye anapeleka citsanzo cangwilo cimene tiyenela kutengela . ( 1 Pet . Ni mautumiki ati amene mtumwi Petulo anapatsidwa ? Nanga anaonetsa bwanji kuti anali wolimba mtima ? Mngeloyo anakamba kuti izi zidzacitika “ pa mapeto a masikuwo . ” ‘ Tiziyesetsa kukhala pa mtendele ndi anthu onse . ’ Anthu opanda ungwilo akakamba zinthu zotelo , timamvetsetsa mmene amvelela , cifukwa ifenso ndife anthu monga io . Awa ni mafunso amene makolo ambili amadzifunsa mwana wawo akawauza kuti afuna kubatizika . ( Mlal . Mkuluyo anakamba kuti anali mneneli wa Yehova . ( Miyambo 27 : 12 ) Monga mmene timatetezela umoyo wathu , tifunika kucita zimene tingathe kuti titeteze maganizo athu ndi mtima wathu . Mwacitsanzo , ngati munthu walumpha mumtengo na kuyesa kumbululuka monga mbalame , akhoza kudzibweletsela mavuto . Zimenezi zikanabweletsa mavuto aakulu pa io ndi mbadwa zao , monga mmene Mulungu anawacenjezela . ( b ) Kodi akulu amene akutumikila m’madela osowa ali ndi udindo wofunika kwambili uti ? Anafika mpaka podzigobela manda olemekezeka , ndiponso anali kukwela pa ‘ magaleta ankhondo aulemelelo . ’ — Yes . Kucokela nthawi imeneyo sitinaonanenso . Patapita zaka zocepa , n’nadabwa kuti anidziŵa pa gulu la anthu pa msonkhano wa cigawo mumzinda wa Toronto , ku Ontario . Anakamba conco pulofesa wina wa mbili yakale na zinthu za moyo , dzina lake William Provine . wolimbikila nchito ? Aisiraeli anaimba nyimbo yacilakiko yotamanda Yehova pambuyo pakuti alanditsidwa mozizwitsa muukapolo ku Iguputo . Nthawi zonse anali kumuuza zimene ayenela kucita . ZOTSATILAPO ZAKE : Baibulo ni buku imene yamasulidwa ndi kufalitsidwa kwambili m’mbili yonse ya anthu , ngakhale kuti mafumu amphamvu ndi abusa a cipembedzo anayesetsa kuti aiwononge . Koma zinali zovuta ngako kwa mwana wakeyo . Olo zinali conco , mtsikanayo anavomela na mtima wonse kucita zimene atate wake anasankha . Informant inalinso na pempho yatsopano yakuti : “ Tifuna gulu la apainiya okwana 1,000 . ” Robert , amene tamuchula m’nkhani yoyamba , ali na maganizo ofanana ndi amenewa . Iye amayesetsa kupewa zinthu zoipa . Iye anati : “ Muzicita zimenezi pondikumbukila . ” — Luka 22 : 19 . Pamene mwana ali wamng’ono , amangoyang’ana atate wake akuyendetsa . Adziŵanso kuti aliyense wa iwo angakhale munthu wabwino . KUTHA KWA NKHONDO , CIWAWA NDI KUPANDA CILUNGAMO . Baibo imati : “ Yehova anapitilizabe kukhala ndi Yosefe ndi kumusonyeza kukoma mtima kosatha . . . Timaonetsa cikondi cimeneci mwa zocita zathu osati mwa mau cabe . Ngati ndinu mkulu , mumadziŵa mmene mungathandizile abale amene apatuka n’kuyamba kulowela njila yolakwika . Davide anali ndi makhalidwe abwino kwambili . ( Yakobo 1 : 17 ) Kodi mukusangalala ndi mapindu amenewa a kupatsa ? Pa njinga yake ananyamula mabulangeti , zovala , zakudya , ndiponso mabuku ambili . Imodzi mwa njila zimenezo ni ufulu wokunkha za m’munda . — Lev . Kodi zonse izi ni kuwamiliza cabe nkhani , koma sizingacitike ? Kodi mfundo zimenezo ndi ziti ? Kodi akulu angatsatile bwanji citsanzo ca Samueli pankhani yophunzitsa ena ? Ziyeneletso zimene io afunikila kukwanilitsa zipezeka pa 1 Timoteyo 3 : 8 - 10 , 12 , 13 . 2 : 15 - 17 ) Mwa kucita zimenezi , io akanacita zonse zimene Mulungu anafuna kuti io acite . Yehova amene ndi “ Woyela ” amafuna kuti odzozedwa ndi a “ nkhosa zina ” azicita zonse zimene angathe kuti akhale oyela m’makhalidwe ao onse . — Yoh . 10 : 16 . Koma anthu ambili m’dzikoli amathela nthawi yoculuka akuceza pa intaneti , ndipo amaceza ndi anthu amene sawadziŵa ngakhale pang’ono . Cifukwa ciani takamba conco ? — Yak . Poona mmene zinthu zinalili ndinaganiza zokathandiza abalewo . ” Cifukwa sizingatheke kuti mau a Yesu asakwanilitsidwe . ’ 34 : 11 - 14 . N’ciani cingakuthandizeni kukhala wocenjela ? Mpaka nyumba zao zitakhala zopanda anthu okhalamo , ndiponso mpaka nthaka itaonongekelatu . ” — Ŵelengani Yesaya 6 : 8 - 11 . Ngati tasoŵelatu cocita , angacititse kuti ena atipatseko zimene ali nazo . Kumvela malangizo a anthu acikulile komanso okhwima mwauzimu , ni cinthu canzelu . Ndiyeno , mokweza ndi momvekela bwino , Maria akuyankha mafunso aŵili amene mkambi wafunsa . Mofanana ndi alongo amenewa , kodi mwina ifenso tingakhale na maganizo a tsankho amene tifunika kuthetsa ? Cikondi ndico kukhudzika mtima ndi munthu amene mumakondwela naye . Ngakhale kuti dzuŵa laloŵa kale , simukuda nkhawa cifukwa muli na toci yamphamvu . Kodi tingawathandize bwanji ‘ kutumikila Yehova mokondwela ’ ngakhale kuti akumana ndi mavuto ? ( Sal . Mtumwi Paulo anafotokoza za cikondi ceniceni . Kodi ndani amene anadziŵa kuti ulosi wa m’Baibo wakwanilitsidwa ? Mwacitsanzo , chimolo lingakhale misece kapena cinyengo . — w16.05 , peji 7 . Pali zifukwa zambili zimene tiyenela kucitila zimenezi . Analidi magaleta a nkhondo ocititsa mantha kuwayandikila . Nayenso munthu amene amaona zinthu zauzimu kukhala zofunika , amadziŵika monga munthu wokonda zinthu zauzimu . Yesu analonjeza kuti Atate wathu wakumwamba ni wokonzeka ‘ kupeleka mzimu woyela kwa amene akum’pempha . ’ Amadzifunsa kuti : ‘ Kodi ana ndi adzukulu athu adzakhala m’dziko limene muli nkhondo , ciwawa , kuonongedwa kwa cilengedwe , kusintha kwa nyengo ndi milili ? ’ Masiku ano , olosela zakutsogolo amaseŵenzetsa makhadi a njuga za matsenga , mipila ya gilasi , tunthu tocitila mayele , na zina za conco pofuna “ kudziŵa ” tsogolo la munthu . “ Yehova Mulungu anati : ‘ Si bwino kuti munthu [ mwamuna ] akhale yekha . Mdyelekezi akadzamasulidwa m’ndende yake adzakhalanso na colinga cosoceletsa anthu . ( Ŵelengani 2 Timoteyo 2 : 19 . ) Kodi pali zinthu zimene zimakusokonezani kucita zinthu zofunika kwambili ? Anali kusangalala kuphunzila mwa njila imeneyi ndipo zinawathandiza kulimba mtima . Iwo anali mtundu wokhawo umene Mulungu anaupatsa ‘ mau ake , malangizo ake ndi zigamulo zake . ’ Koma kucita ciwelewele kukanawalepheletsa kulandila kukoma mtimako . KUTANGOTSALA kanthawi kocepa kuti Aisiraeli aloŵe m’Dziko Lolonjezedwa , amuna ambili aciisiraeli anacita “ ciwelewele ndi akazi a ku Mowabu . ” 10 : 1 , 2 ) Ndiyeno ganizilaninso zimene Mulungu anauza Aroni . Lamba imeneyo inali kuthandiza kuti msilikaliyo asamamvele kulema kwambili akavala codzitetezela pacifuwa . Miyambo 3 : 11 , 12 imati : “ Mwana wanga , usakane malangizo a Yehova , . . . cifukwa Yehova amadzudzula munthu amene amam’konda . ” Koma ngati mwayesedwa kuti muphwanye lamulo linalake la Yehova , ganizilani mavuto auzimu amene mungakumane nawo cifukwa colephela kudziletsa ku zilakolako zoipa . Iye anati : “ Lemekezani anthu , kaya akhale amtundu wotani . Muzim’khululukila mnzanu wa m’cikwati , podziwa kuti “ tonsefe timapunthwa nthawi zambili . ” — Yakobo 3 : 2 . Sitiyenela kunyalanyaza nchito yosamalila Nyumba ya Ufumu ( Onani ndime 16 ndi 18 ) Tiphunzilapo ciani pa mau a Yesu opezeka pa Mateyu 28 : 19 , 20 ? ( Yos . 2 : 9 - 11 ) Zocitika zimenezi zimaonetsa kuti Yehova ali na mphamvu ndipo amatikonda . Kodi umabala tummela tung’ono - tung’ono twa tiligu ? M’baleyu anali kutumikila m’Dipatimenti ya Utumiki , ndipo mu 1998 anaikidwa kukhala wothandiza m’Komiti Yoona za Atumiki a pa Beteli ya Bungwe Lolamulila . 3 / 1 Kodi mungacite zinthu ziti kuti mulimbitse mgwilizano m’cikwati canu ? N’ciani cinathandiza Danieli kukhalabe wolimba mwauzimu pamene anali kukhala kudziko lacilendo ? Nanga munanimangilanji ? ” Magaziniyo inakamba kuti abale a Kristu adzakhala akulamulila ndi iye kumwamba panthawi ya Ulamulilo wa Zaka 1000 , ndipo sadzalandila thandizo kucokela kwa anthu amene adzakhala padziko lapansi . Anapitiliza kudziphunzitsa . Kalata imodzi yolembedwa ndi Paulo sinalembedwe m’Baibulo . Kodi pali zifukwa zotani zokhulupilila kuti iye anaukitsidwa kwa akufa ? ( Aroma 2 : 29 ) Pocita nao pangano latsopano , Mulungu anali kudzaika ‘ malamulo ake m’maganizo mwao ndi kuwalemba m’mitima yao . ’ ( Aheb . Mungacite zimenezi mwa kuonetsa mzimu wodzimana . Conco , nthawi zonse tikakumana ndi mavuto , ni bwino kumaganizila za kufunika kocilikiza ulamulilo wa Mulungu . Pofuna kutithandiza kuti tiziwaona moyenelela , tikambilana mmene Yehova amasankhila anthu amene afuna kuwaumba , cifukwa cake amawaumba , ndi mmene amawaumbila . Izi zinacititsa kuti Mirjeta azivutika kulalikila anthu a ku Serbia . Iye anaona kuti afunika kucitapo kanthu kuti athetse maganizo olakwika amenewa . Bungwe Lolamulila la m’nthawi ya atumwi linali kulimbikitsa abale amene anali kutsogolela mu mpingo komanso Akhristu ena onse . YEHOVA anatipatsa nzelu zotithandiza kuganizila mmene ena akumvela . Kodi zocitika ziŵilizi zikusiyana motani ? Ife tidziŵa kuti Yehova amaona zonse zimene timacita . Anauza amayi kuti cifukwa cakuti n’nali kugwilizana ndi a Mboni , sin’nali kupeleka citsanzo cabwino kwa ana a sukulu anzanga . Nthawi zina , angelo otumidwa na Mulungu anali kuloŵelelapo pa zocitika za mpingo wacikhristu woyambilila . Anali kucita izi kukakhala kofunikila kuti akwanilitse cifunilo ca Yehova . Nanga n’cifukwa ciani timadedwa ngakhale kuti ndife anthu oona mtima , a makhalidwe abwino , ndi otsatila malamulo ? Ofalitsa a ku maiko ena amene anagwilako nchito yapadelayi anafotokoza mmene inakhudzila utumiki wawo atabwelela kwawo . Ine ndi cisumbali canga tinazindikila kuti tifunika kulembetsa ukwati wathu ku boma . Cimeneci sicikanakhala ciyeso cacikulu ngati Satana anayesa Yesu pogwilitsila nchito masomphenya . Komabe , anzathu amaphatikizapo mkazi kapena mwamuna wathu , abale ndi alongo mumpingo , ndi anthu amene timakumana nao mu ulaliki . Cisangalalo cimene timakhala naco pothandiza kukongoletsa paladaiso wauzimu , cimaonetsa cisangalalo cacikulu cimene tidzakhala naco mtsogolo pokonza paladaiso weniweni pano padziko lapansi . MAKOPE 18,400,000 Iwo amadziikila zolinga zimene angakwanitse . Komanso , m’bale wina wa ku Philippines anati : “ Kukhala munthu wauzimu kwanithandiza kukhala na mtendele wa m’maganizo . Pezani cimwemwe potumikila ena . ( 1 Akorinto 1 : 10 ) Uthenga waukulu umene umapezeka m’magazini yakuti Nsanja ya Mlonda , Imalengeza za Ufumu wa Yehova , ndi wonena za Ufumu wa Mulungu . Patapita nthawi iwo anabatizika . Satana amasangalala mtumiki wa Yehova akacita chimo ( Onani ndime 10 ) Apa n’zoonekelatu kuti Yehova amaona kuti makhalidwe amenewa ni ofunika kwambili kuposa cuma ca kuthupi . Onani zifukwa zitatu zotsatilazi . Iye anali kuwaona kamodzi pa caka akaloŵa m’malo oyelawo pa Tsiku la Mwambo Wophimba Macimo . ( Aheb . Iye amatiumba moleza mtima mwa kutipatsa malangizo , ndipo amatiyang’anila kuti aone ngati tikuwatsatila kapena ai . Kuyambila pa November 1 , 1999 , Nyumba za Ufumu zokongola zoposa pa 28,000 zamangidwa pa dziko lonse . ( b ) Kodi acicepele angacite ciani kuti apewe kutengela zocita za anzawo ? N’cifukwa cake Paulo asanakambe mau a pa 1 Akorinto 10 : 29 , anati : “ Zinthu zonse ndi zololeka , koma si zonse zimene zili zaphindu . Komabe , tinapitiliza kuika zinthu za Ufumu patsogolo . — Mat . Monga taonela , Satana ndi wamphamvu , wankhanza , ndi wacinyengo . Anasintha umoyo wawo , ndipo akuyembekezela tsogolo labwino . ( Akol . Makolo acikristu naonso ali monga abusa , ndipo ayenela kukhala ndi makhalidwe amene m’busa weniweni amakhala nao . Fanizo limeneli linawayenelela kwambili pa msinkhu wawo . Kucokela kale , atumiki a Yehova akhala akudziŵa kuti Akhiristu sayenela kumenya nkhondo . Onani New World Translation of the Holy Scriptures — With References , Zakumapeto 1A “ Dzina la Mulungu m’Malemba Aciheberi , ” tsamba 1561 . Ngakhale pamene Mfumu Davide anali wokalamba , anayesetsa kulimbikitsa kulambila koona . Njila imodzi imene iye akucitila zimenezi ndi kudzela m’Sukulu ya Ulaliki . Timasangalala kuona acinyamata ambili akubatizidwa caka ciliconse . ( Aroma 5 : 12 ; 6 : 23 ) Ngati Yesu sanauke , nafenso tingakambe kuti : “ Tiyeni tidye ndi kumwa , pakuti maŵa tifa . ” ( 1 Akor . Mwacitsanzo , mpainiya wina wa ku New York City , dzina lake Eddie , anali kucita mantha kukambilana ndi anthu . Cikwati cimalimba ngati amuna ndi akazi ‘ apitiliza kulolelana ndi kukhululukilana ndi mtima wonse . ’ CIFUKWA CAKE ENA AMAKAIKILA : Anthu ambili amene amakhulupilila Mulungu amaona kuti iye ali patali ndi io . Acicepele ambili aona kuti ngati akonzekela bwino ulaliki , zimakhala zosavuta kulalikila uthenga wabwino kwa ena . ( Aef . 4 : 8 , 11 - 13 ) Tingacite ciani kuti tipindule na mphatso zimenezi ? Timaona kuti ni mwayi kudziŵa Yehova komanso kukhala na ufulu umene kulambila koona kumabweletsa . ( 1 Tim . 3 : 2 , 12 ) Pokhala “ thupi limodzi , ” a m’cikwati afunika kuphatikana pamodzi , ndi kulola cikondi cawo kwa Mulungu ndi kwa wina na mnzake kulimbitsa cikwati cawo . MBILI : KUSAKHULUPILILA KUTI KULI MULUNGU N’cifukwa cake mtumwi Petulo analemba kuti : “ Ngati anthu akukunyozani cifukwa ca dzina la Kristu , ndinu odala cifukwa . . . mzimu wa Mulungu , wakhazikika pa inu . ” — 1 Pet . “ [ Abulahamu ] anachedwa ‘ bwenzi la Yehova . ’ ” — YAK . NKHANI YA PACIKUTO ( Onani pikica kuciyambi . ) ( b ) Malinga ndi Akolose 3 : 5 - 9 , ni makhalidwe ati amene ali mbali ya umunthu wakale ? Kodi tiyenela kukumbukila ciani ngati acibululu akutitsutsa cifukwa colambila Yehova ? Monga mmene taphunzilila m’fanizo la nkhosa ndi mbuzi , “ nkhosa ” zidzathandiza abale a Yesu . Cifukwa cina cacikulu cimene timapitilizila kulalikila n’cakuti timakonda anthu anzathu . ( Mat . YEHOVA anapatsa ena moyo n’colinga cakuti iwonso azisangalala . Iye analenga angelo , ndipo m’kupita kwa nthawi analenganso anthu . Koma Yehova sanyalanyaza macimo . Kuti azitumikila bwino , wolambila Yehova aliyense afunika kukhala na cizoloŵezi cophunzila Baibulo . Kodi nzelu zocokela kwa Mulungu timazipeza bwanji ? Iye analembela Akhristu a ku Roma kuti : “ Ndikulakalaka kukuonani kuti ndikugaŵileni mphatso inayake yauzimu kuti mukhale olimba , kapena kuti tidzalimbikitsane mwa cikhulupililo , canu ndi canga . ” Asa analimbikitsa ena kulambila Yehova . Atumiki anthawi zonse aphunzila makhalidwe ndi maluso amene ndi ofunika tsopano ndiponso m’dziko latsopano . Zinthu zinali zovuta mu umoyo wake , mofanana ndi mmene zilili kwa ambili a ise masiku ano . Ngati onse aŵili amasonyezana cikondi , kudzakhala kosavuta kwa io kukhutilitsa zosoŵa za m’maganizo ndi za kuthupi za mnzao . Ngati alibe zolinga zenizeni muthandizeni kupanga zolinga zabwino zimene angakwanitse . Sitikaikila kuti madalitso onsewa tidzawapeza cifukwa cakuti Yesu anati : “ zinthu zonse n’zotheka kwa Mulungu . ” Caciŵili , tiyenela kuganizila zimene tingacite kuti titengele citsanzo ca Mulungu ndiponso mapindu amene tingapeze ngati tacita zimenezi . Wadela amapendanso umoyo wauzimu wa banja la m’bale amene akulingalilidwa . Conco , tiziuzako ena coonadi ca Ufumu cimeneci mwacangu . — Mat . Atagwidwa ndi cifundo cacikulu , Yosefe anacoka n’kupita kwayekha kukalila . ( Gen . Mmodzi wa io anali namwali Mariya . Conco , anthu a Mulungu anafunika kukumbutsidwa kuti abwelele kwa Yehova na kuleka kuika patsogolo zofuna zawo . A Mboni za Yehova ananilandila mosasamala kanthu za mmene umoyo wanga unalili . Mwacitsanzo , anthu ena osauka amaganizila kuti adzalemela kwambili ndi kukhala opanda mavuto . ( a ) Kodi otsatila a Yesu anali monga ana m’njila yotani ? 73 : 12 - 17 ; 143 : 10 . Mlongo wina dzina lake Shari anati : “ Kaŵilikaŵili apainiya amene sali pa banja akacoka mu ulaliki amakhala okha . Atsogoleri a sunagoge kumeneko anawauza kuti : “ Amuna inu , abale athu , ngati muli ndi mau alionse olimbikitsa nawo anthu , lankhulani . ” Mwacitsanzo , iye analamula kuti munthu safunika kupha mnzake . Pamene mapeto a dongosolo lino ali pafupi kwambili , ndife oyamikila kuti Yehova pang’onopang’ono watithandiza kumvetsa fanizoli , ndi mafanizo ena opezeka pa Mateyu caputala 24 ndi 25 . Cifukwa cakuti iye sanafune ‘ kumangidwa m’goli ’ ndi wosakhulupilila . N’ciani cimene cinam’cititsa kukhala ndi cimwemwe ? Baibulo limati “ maso odzikweza ndi mtima wodzikuza ndizo nyale ya anthu oipa , ndipo zimenezi ndi chimo . ” — Miy . N’tangoyamba , n’naphunzila kuti dzina leni - leni la Mulungu Wamphamvuyonse ni Yehova . Tingacite ciani kuti tithandize anthu kulemekeza Baibo pamene tilalikila ? 7 , 8 . ( a ) N’cifukwa ciani anamwali anzelu anali okonzeka ? Uyenela kucita bwanji kuti ukambilane bwino za cilengedwe kapena za Baibulo na anzako a kusukulu , matica , ndi ena ? Tinali kucita utumiki wathu wa umishonali mu mzinda wa Campos , mmene tsopano muli mipingo 15 . 5 : 19 , 30 ) Popeza kuti Yesu anali wodzicepetsa na womvela , anthu a mitima yabwino anali kumasuka naye . Tingacitenso bwino kukumbukila zimene Paulo anacita monga “ ciwiya [ ca Khristu ] cocita kusankhidwa cotengela dzina [ la Yesu ] kupita nalo kwa anthu a mitundu ina . ” ( Mac . Mwacionekele , iwo anakondwela kudziŵa kuti Paulo anali kuwaganizila . Malamulo na mfundo za m’Mau a Mulungu ‘ n’zopindulitsa pa kuphunzitsa , kudzudzula , kuwongola zinthu ndi kulangiza m’cilungamo . ’ ( 2 Tim . Iwo adzaukitsidwa ndipo adzakhala na moyo wosatha m’paradaiso , pano padziko lapansi . — Luka 23 : 43 . ( Aefeso 5 : 25 ) Zoonadi , ngakhale kuti Yesu Kristu sanakwatilepo , citsanzo cake cingakuthandizeni kukhala mwamuna wabwino . ULOSI woyamba kulembedwa m’Baibulo ndi wofunika kwambili pa kukwanilitsidwa kwa colinga ca Yehova . Komanso tikalakwa , cidzatisonkhezela kulapa na mtima wonse . Mulungu “ adzapukuta misozi yonse m’maso [ mwathu ] . ” Cifukwa cimodzi cinali cakuti Yakobo anali kukonda kwambili Yosefe , ndipo anamupatsa mkanjo wapadela . Kodi Baibulo limafotokoza kuti cidzacitika n’ciani panthawiyo ? Yosefe ayenela kuti analimbikitsidwa kwambili cifukwa codziŵa kuti Yehova anali naye nthawi zonse . Nthawi zambili , munthu wakuthupi amafunitsitsa kukhala wochuka , amakonda kufuna - funa zinthu zakuthupi , ndiponso amaumilila kuteteza ufulu wake . Mofanana ndi mmene mkanjo wapadela wa Yosefe unalili , khalidwe la Akristu oona , liyenela kukhala losiyana ndi la anthu owazungulila . Ngakhale n’conco , iwo analamula kuti mafupa ake afukulidwe . Mafupawo anawatentha , ndipo phulusa lake anakalitaya mumtsinje wochedwa Swift . Zimene anacitazo zinali zanzelu cifukwa pa tsikulo Aisiraeli masauzande anaphedwa cifukwa ca kulambila fano . Munthu amene wadzozedwa angadzifunse kuti , ‘ N’cifukwa ciani Yehova wasankha ine osati munthu wina ? ’ Iye ni “ Yehova mmodzi . ” — Deuteronomo 4 : 35 , 39 . Yesu anayambitsa mwambo umene umacitika caka ciliconse pofuna kutikumbutsa za mphatso ya dipo . ( 1 Pet . 3 : 7 ) N’zoona kuti si nthawi zonse pamene mwamuna angatsatile malingalilo a mkazi wake . Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani ? — Aka ni kabuku ka mapeji 32 kamene kamafotokoza mwacidule mfundo yaikulu ya m’Baibo Akulu - akulu a boma ali na udindo wolimbikitsa anthu kutsatila malamulo ndi kukhala mwamtendele , ndiponso kusamalila nzika za dziko lawo . Ganizilani mapindu atatu awa : Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika , lili na dzina lopatulika la Mulungu lakuti Yehova m’Malemba a Ciheberi na m’Malemba Acigiriki Acikhristu . 30 : 18 . Koma kodi kucita zimenezi kumawathandiza kupezadi ufulu ? Izi zitanthauza kuti Yehova amaona nyenyezi iliyonse kukhala yapadela . ( 1 Akor . Rodney anati : “ Tinakhudzidwa kwambili titaona njala yauzimu imene anthu kuno ali nayo . Munthu aliyense amakhala ndi malile ocita zinthu . 13 : 37 , 38 ) Iwo adzadindidwa cidindo comaliza cisautso cacikulu cisanayambe . ( Chiv . Timafunikila kutsatila miyezo yake ya makhalidwe abwino . NYIMBO : 10 , 2 6 : 44 ) Kodi muganiza kuti na imwe munakokedwa na Mulungu ? Mungaonenso Chivumbulutso 14 : 1 , 3 . ( Mateyu 16 : 21 - 27 ) Apa Petulo anaphunzila mfundo yosaiŵalika . — 1 Petulo 2 : 20 , 21 . 64 : 4 . Yehova Mulungu wake , ndi amene anamuuza kumenya nkhondo imeneyi , ndipo ananenelatu kuti mkazi ndi amene adzathetsa nkhondoyi . Masiku anonso , Yehova akhoza kuwayesa olungama Akhiristu okhulupilika amene ali na ciyembekezo ca m’Baibo codzakhala na moyo wamuyaya padziko lapansi . Enanso amapatsa cifukwa cofuna kuti wolandilayo aziwacitila zinthu zabwino , kapena cifukwa cofuna kuti nayenso awapatse cinacake . Angacite zimenezi mwa kulemekeza makolo awo ndi kuwathandiza pa zinthu zakuthupi . 28 : 6 . Baibo imaonetsa kuti pambuyo pake , Paulo na Maliko anatumikilanso pamodzi . Yehova anan’thandiza pa vuto iliyonse . ” Nthawi zina munthu angakambe zinthu zotikhumudwitsa . Sankhani mabwenzi amene adzakulimbikitsani kukhala na zolinga zauzimu ndi kupewa mavuto . Pamene tikukumana ndi mavuto amenewa , kodi tingapilile bwanji ndi kukhalabe pa ubwenzi wolimba ndi Mulungu ? N’ciani cingakuthandizeni ? Angelo amenewo amadela nkhawa za ife ndi zocita zathu . ( 1 Pet . Ndi zinthu zitatu ziti zimene tiyenela kucita kuti tizimvetsetsa mafanizo a Yesu ? Ngati n’conco , mungayambe makambilano anu mwa kufunsa kuti : “ Ndi ndalama zingati zimene mwamuna ayenela kukhala nazo kuti banja lake likhale lacimwemwe ? ” Mulungu adzaletsa “ nkhondo mpaka kumalekezelo a dziko lapansi ” kudzela mwa Yesu , amene ndi “ Kalonga Wamtendele . ” Kodi kuganizila udindo wa Yesu monga Wotiombola na Mkulu wa Ansembe kungatithandize bwanji kukhulupilila kuti Mulungu angaticitile cifundo ? 6 : 5 ) Zimene Mose anasankha zinam’thandiza kupewa mavuto aakulu . Kodi mau a Paulo amawakhudza bwanji ? Mboni za Yehova kudela lanu n’zokonzeka kukuthandizani kupeza cidziŵitso cimeneci . Nthawi zina tinali kukhala munsi mwa thebulo ya nsimbi imene anaipanga n’colinga cakuti iziwateteza ngati nyumba yagwa . N’cifukwa ciani Yehova ndi woyenela kumuyamikila ? A Inoki : Ndikuona kuti ndinu munthu womasuka . Kodi ndi nthawi iti imene anthu amapezeka panyumba m’gawo lathu ? Kodi munthu wodzicepetsa amaganizila ciani pofuna kupita patsogolo mwauzimu ? ( Aroma 13 : 8 - 10 ) Atumiki a Mulungu amakonda anzao ndi mtima wonse ngakhale kuti akukhala m’dziko limene likulamulidwa ndi Satana , lodzala ndi magaŵano , ciwawa , ndi zinthu zoipa . Anthu ena amaganiza kuti nkhani ya Davide ndi Goliyati ni nthano cabe . Kupitila m’dipo , Mulungu anapeleka mwayi kwa onse amene amaonetsa cikhulupililo wakuti akhalenso angwilo , ndi kukhala ndi moyo kwamuyaya . Koma Mulungu amasangalala ngati timacita zimene tingathe mosangalala . — Mat . ( a ) N’cifukwa ninji lemba la caka ca 2017 n’loyeneleladi ? Ili ndilo tsamba loyambilila . Kodi colinga cimene analengela zinthu zonsezi cinali ciani ? Koma iwo anayankha mafunso anga onse moleza mtima komanso momveka bwino kucokela m’Baibo . ( 1 Yohane 4 : 9 ) Mfundo imeneyi ipangitsa dipo kukhala mphatso yamtengo wapatali . Panthawi imeneyo sitidzayenela kulola cina ciliconse kutigaŵanitsa . Ndiye cifukwa cake Paulo anati : “ Sizingatheke kuti muzimwa za m’kapu ya Yehova komanso za m’kapu ya ziwanda . Cikumbumtima ndi umunthu wamkati umene umatithandiza kuzindikila cabwino ndi coipa . Inde ! 9 , 10 . ( a ) N’cifukwa ciani anthu anali kupita kudziwe la Betesida ? Pankhani yolemekeza ena , kodi Mboni za Yehova zimasiyana bwanji na anthu ena ? ( Aefeso 5 : 33 ) Eee ! Ndipo ngakhale nkhondoyo isanayambe , io anali atamangidwapo ndi apolisi akabisila a ku Germany ( Gestapo ) , ndi kuwatumiza ku msasa wa cibalo ku Lichtenburg . N’cifukwa ciani Kalebe ndi Yoswa anali ndi cikhulupililo colimba ? Paulo anawonjezela kuti : “ Pakuti Mulungu anati : ‘ Sindidzakusiyani kapena kukutayani ngakhale pang’ono . ’ Kodi kusintha zinthu zina m’nyumba yao , kudzathandiza kuti makolo aziyenda , azisamba , ndi kucita zinthu zina popanda vuto ? 6 : 25 - 27 . Ŵelengani Salimo 45 : 1 , 17 . Kucotsa munthu wosalapa mumpingo kumabweletsa madalitso okhalitsa kwa onse , kuphatikizapo kwa wolakwayo , ngakhale kuti poyamba cilangoco cimakhala coŵaŵa . Kuti akulu adziŵe ngati munthu ni wolapadi , afunika kupenda kaonedwe kake ka zinthu , kaimidwe ka maganizo ake , na mmene mtima wake ulili . ( Chiv . M’bale Mumba : Zikomo . N’cifukwa ciani mtumwi Paulo analangiza Akhristu oyambilila aciheberi kuti awonjezele mzimu wolimbikitsana ? 109 - 112 . Komabe , abale na alongo athu amene amalalikila m’madela okhala na Mboni zambili conco amakumana na mavuto ena apadela . TSIKU lina m’maŵa , Mkulu wa Ansembe Aroni anaimilila pakhomo la cihema ca Yehova , atanyamula nsembe yofukiza m’cofukizila nsembe . M’nkhani yapita , tinakambilana njila zinai zimene Yehova waonetsela cikondi cake cacikulu kwa ana ake . Iwo angamuone kuti alibe cikondi ndi kuti ndi wodzikonda . Tinamuyamikila kwambili Yehova . Kodi ndimafunitsitsa kulalikila ena kapena sindimalalikila pa zifukwa zosamveka ? kufunika kwakuti wocimwa acitepo kanthu mwamsanga kuti Mulungu amucitile cifundo ? 17 : 3 ) Pogwilitsila nchito gulu lake , Atate wathu wakumwamba amatipatsa cakudya ca kuuzimu coculuka ndi colimbikitsa . Kufatsa kungabweze mkwiyo . Cikumbumtima : Cikumbumtima ndi umunthu wamkati umene umatithandiza kuzindikila cabwino ndi coipa . Tingaphunzile zambili kwa Eliya amene anali ndi cikhulupililo camphamvu pamene anali kulimbana ndi zinthu zopanda cilungamo . ( Mateyu 24 : 14 ; 28 : 19 , 20 ) Izi zitanthauza kuti uthenga wabwino uyenela kulalikidwa padziko lonse . 15 : 21 , 22 . Mwacitsanzo asanapatse atumwi ake nchito yopanga ophunzila , Yesu anawauza cifukwa cake anafunika kugwila nchito imeneyo . Mateyu 24 : 7 : “ Kudzakhala njala . ” Koma zimene Yesu anauza Akhiristu a ku Tiyatira zionetsa kuti kuchula cimene tikuyamikila ndiye kumathandiza kwambili . Nikotini amacititsa munthu kukhala wocangamuka ndi wosakondwa . “ Ukakabatizika cabe , ndiye kudzakhala kutha kwa cikwati na ine ! ” Iwo akuyembekezela kudzalandila mphoto ya moyo wosatha pano padziko lapansi . Cimeneci ni ciyembekezo cokondweletsa ngako ! — 2 Pet . Masiku ano , zimene Mateyu na Luka analemba zokhudza mzela wa Yesu wobadwila zimalimbitsa cikhulupililo cathu ndipo zimatithandiza kutsimikizila kuti malonjezo onse a Mulungu adzakwanilitsidwa . ( Salimo 130 : 3 ) Tingatengele Yehova mwa kuona abale athu mmene iye amawaonela . Nyimbo za kumwamba zimene zikuimbidwa m’bwalo la mfumu zikupangitsa mkwatiyo kusangalala kwambili poganizila kuti mwambo wa cikwati cake wayandikila . Conco , pemphelo langa tsiku lililonse linali lakuti Mulungu ‘ atipatse cakudya cathu calelo , ’ kuti tikhale ndi moyo . Iye anena kuti popeza kuti Farao analota kaŵili malotowo , ndiye kuti Yehova anatsimikiza mtima kucita zimenezo . Ana a Isiraeli aculuka kwambili ndipo ndi amphamvu kuposa ife . ’ Mungaonetse bwanji kuti mucilikiza gulu la Yehova kwathunthu ? Nili na umoyo wabwino ndipo nimadziŵa kuti Yehova ananikhululukila ndipo akunicilikiza . Yesu anali kudziŵa kuti Petulo amamukonda , koma anadziŵanso kuti apa iye waganiza molakwika . Iye anati : “ Kunanithandizadi . Koma kodi timakhulupilila kuti Yehova amatikonda ? Cinanso , kupatsa ni mbali ya kulambila Yehova . Iye analonjeza kuti adzapita kukakamba na kampani ya inshuwalansi ya Luigi kuti imukonzele mwamsanga motoka . Zimene afufuza zaonetsanso kuti ngati munthu amene ayesa - yesa kuti aleke kumwa moŵa athandiza ena , amacepetsako nkhawa . Akhozanso kudziletsa ngati wamvela cilaka cakuti amwe moŵa . 5 : 19 . Kaya mukukumana ndi mavuto otani polalikila uthenga wabwino , dziŵani kuti Yehova angakuthandizeni kuwagonjetsa . Cikhulupililo cimatithandiza kuona “ umboni wooneka wa zinthu zenizeni , ngakhale kuti n’zosaoneka . ” ( Aheb . Na ise n’cimodzi - modzi . Malinga ngati tikhalabe ogwilizana na Khristu mwa kutsatila mapazi ake mosamala , tidzakhala na cimwemwe monga cimene iye amakhala naco pocita cifunilo ca Atate ake . ( Yoh . 4 : 34 ; 17 : 13 ; 1 Pet . Kodi lemba la Mateyu 6 : 33 limatithandiza bwanji pamene ticita zosangulutsa ? Baibulo limayelekezela Satana ndi mkango wobangula umene ukuŵendelela nyama . Iye analukamba za anthu osumika maganizo na mtima wawo wonse pa zolakalaka ndi zofuna za thupi lopanda ungwilo . Mukatelo , “ mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu . ” Tiyenela kumva bwanji poona kuti Mulungu anakonza njila yotimasula ku ucimo ndi imfa ? Cifukwa cakuti ndife opanda ungwilo ndipo tinatengela mzimu wosayamikila kwa makolo athu oyamba . 3 : 14 . N’cifukwa ciani kukumbukila mfundo imeneyi n’kofunika ? Nditamufunsa funso limeneli , anazindikila kuti ndinali kukamba zoona cifukwa nkhope yake inagwa . Zocita zawo ndi kaganizidwe kawo zinali kuonetsa kuti anali kukonda kwambili Yehova . Iye analeledwa m’coonadi ndi makolo ake kuyambila ali ndi zaka zisanu . Akhristuwo anali kufunikila cilimbikitso na citsogozo cifukwa anthu anali kuwatsutsa na kuwanyoza . N’ciani cingakuthandizeni kuti musamadziimbe mlandu ? Mwacitsanzo , makopotala ( apainiya ) atalangizidwa kuti asamacite malonda pogwila nchito yolalikila , kopotala wina anakhumudwa n’kuleka coonadi ndipo anayambitsa kagulu kake ka ophunzila Baibo . Wodwalayo akamwalila , zingakhale bwino kudziŵitsa mnzanu wodalilika amene anavomela kukuthandizani . “ [ Yesu ] ndiye cifanizilo ca Mulungu wosaonekayo , woyamba kubadwa wa cilengedwe conse . ” — Akolose 1 : 15 . Conco , tingakhale otsimikiza kuti iye amamvela na kuyankha ‘ madandaulo athu . ’ — Sal . Tuakacisi twina tunamangidwa pamalo amene panacitikila cinthu cina cochulidwa m’Baibulo , kapena pamalo amene akuganizila kuti panacitikila “ zozizwitsa ” zinazake posacedwapa . Nanga anacita zimenezo kufika pati ? Pamsonkhano wa bungwe lolamulila la Akristu a m’nthawi ya atumwi umene unacitika mu 49 C.E . , wophunzila Yakobo anati : “ Sumeoni [ Petulo ] wafotokoza bwino mmene Mulungu anaceukila anthu a mitundu ina kwa nthawi yoyamba , kuti mwa io atengemo anthu odziŵika ndi dzina lake . ” ( Mac . Panthawiyo ndinaona kuti kwanga kwatha , ndikufa basi . Cioneka kuti Yosefe analipo pamene Yesu anafa . Kodi mipukutu imeneyo inapulumuka bwanji kuti isawonongeke ? Nanga inapulumuka bwanji kwa anthu otsutsa ndi ofuna kusintha uthenga wake ? Yehova akutiphunzitsa kukhala ogwilizana lelolino n’colinga cakuti tidzakhale ogwilizana kwamuyaya . Yehova adzamuteteza ndi kumusunga ali wamoyo . ” ( Salimo 41 : 1 , 2 ) Apa Davide sanatanthauze kuti munthu wabwino amene amaganizila munthu wonyozeka sangafe . Mosakaikila , aneba ake anali kum’funsa cifukwa cake anali kupanga combo cacikuluco . Nora anapita kukatumikila ku mzinda wina , koma ine n’napitiliza kucilikiza nchito yolalikila ku Angat . Malemba ambili amaonetsa kuti dzina la Mulungu n’lofunika kwambili ndi kuti tifunika kulilemekeza . Zida zimenezo zimatithandiza ‘ kuona ’ Mlengi wathu ndi maso athu a cikhulupililo . Yesu Khristu anaphunzitsa mfundo zofunika kwambili zokhudza banja . 135 : 4 ) Komanso buku la Hoseya linakambilatu kuti m’tsogolo anthu ena amene si Aisiraeli adzakhala anthu a Yehova . Komabe , sitifunika kulola ciliconse , kaya nchito kapena maudindo athu , kusokoneza pulogilamu yathu yoŵelenga Baibo . Anati : ‘ N’kuyamba mu umoyo wanga kumvela kuti Mulungu dzina lake ni Yehova . Kodi nimacita bwanji nikakumana na ciyeso ? Cifukwa ca maganizo athu ndi kukwiya , tingakambe mau ndi kucita zinthu zimene pambuyo pake tingamve nazo kuipa . Kenako tinauzidwa kuti tikaonekela kwa waciŵili wa woyang’anila ndendeyo . Tinali kuganiza kuti basi adzatiwonjezela zaka zokhala m’ndende . Zimenezi zinacititsa kuti ‘ dziko lapansi liipe pamaso pa Mulungu woona , ndi kudzaza ndi ciwawa . ’ ( Num . 18 : 21 ) Mofananamo , Yesu na atumwi ake analandila thandizo kwa azimayi ‘ amene anali kutumikila iwo pogwilitsa nchito cuma cawo . ’ — Luka 8 : 1 - 3 . Malemba amatilangiza mobwelezabweleza kuti ‘ tizisamalilana mofanana , ’ ‘ tikhale ndi cikondi ceniceni , ’ ‘ tizitonthozana , ’ ndi ‘ kulimbikitsana . ’ ( 1 Akor . 12 : 25 ; Aroma 12 : 10 ; 1 Ates . ( c ) Ni mphatso ziti zimene zimatilimbikitsa masiku ano ? N’cifukwa ciani tiyenela kuŵelenga mapemphelo olembedwa m’Baibulo ? Capakati pa zaka za m’ma 1400 , kuwala kwauzimu kunayamba kuonekela pang’ono - pang’ono pa zifukwa ziŵili izi : Coyamba cinali kupangidwa kwa mashini opulinthila mabuku . Mwacitsanzo , pamene Paulo anatumiza moni kwa Akristu a ku Kolose , iye anakamba kuti “ amenewa andithandiza ndi kundilimbikitsa ” kwambili . ( Akol . Kupeleka thandizo kwa abale athu ovutika ni njila imodzi yoonetsela kuti timawakonda , ndipo ndise oceleza ( Onani palagilafu 12 ) Zofooka zathu zingatilepheletse kukhala maso . Nkhaniyi iyankha mafunso amenewa . Ifotokozanso zinthu zina zimene tingacite pa nyengo ya Cikumbutso . N’zoona kuti nthawi zina timaona kuti sitingakwanitse kupilila . ( Luka 23 : 18 - 23 ) Inde , iwo ndiwo anacititsa kuti Yesu aphedwe . 7 : 58 - 60 ) Ngakhale n’conco , Milan anafotokoza mmene anamvelela na zimene zinacitikazo . “ Mudzakhala Mboni Zanga ” Izi zinathandizanso a m’banjali kudziŵa mwamsanga maina a abale na alongo . Iwo anali kulambila Baala , ndipo sanali kulemekeza Yehova ndi malamulo ake . Buku lochedwa Encyclopedia of Ancient Rome limakamba kuti : “ Mu ufumu wa Aroma munali madela ena ocepa amene anali pa cidani cacikulu na Aroma . Limodzi mwa madelawo linali Yudeya . Odalitsa iwe ndidzawadalitsa , ndipo otembelela iwe ndidzawatembelela . Mabanja onse a padziko lapansi adzapeza madalitso cifukwa ca iwe . ” ( Gen . Iye amayembekezela zinthu zimene safuna . ( 1 Pet . 2 : 21 ) Dela limene n’napatsidwa linali cigawo cacikulu cochedwa central Luzon . Mkazi anali mphatso ya Adamu yocokela kwa Mulungu , ndipo anali mthandizi wabwino . ( Salimo 25 : 4 , 5 ) Ngati taphunzila cinacake cokhudza Yehova , tiyenela kuganizila mmene tingagwilitsile nchito zimene taphunzilazo . Mtsikanayo anati : “ Ndinadabwa kwambili ! Hutter anaphunzila vitundu va kumaiko a kum’mawa kwa Asia pa Yunivesite ya Lutheran m’tauni ya Jena . Davide anaona kuti Goliyati anali kucita cinthu cina coipa kwambili kuposa kucititsa manyazi gulu la asilikali a Aisiraeli . Anaona kuti anali kunyoza Yehova , Mulungu wa Isiraeli . 22 : 42 . 10 : 16 ; Zek . 8 : 23 ) Pa nthawi ino , magulu aŵiliwa akutumikila mogwilizana motsogoleledwa na Mfumu imodzi yaulemelelo , Yesu Khristu , amene mu ulosi wa Ezekieli akuchedwa “ mtumiki [ wa Mulungu ] Davide . ” Munthu amene amadziŵa njila za Yehova , amadziŵanso kuti iye nthawi zonse amalanga munthu “ pa mlingo woyenela . ” Ndipo n’zimene anacita . Fuko la Efuraimu ndiye inali fuko la mphamvu kwambili pa mafuko 10 a ufumu wa Isiraeli wakumpoto . Ndipo ngakhale Yerobowamu mfumu yoyamba kulamulila ufumu umenewo anacokela ku fuko la Efuraimu . Iye anakamba kuti : “ Nthawi zambili tinali kuyamba ndi mau akuti , ‘ Kodi mungakonde kuŵelenga kapepala aka ? ’ Kuposa olemba onse a Baibo , Yohane anaseŵenzetsa velebu ya Cigiriki imene nthawi zina imamasulidwa kuti kuonetsa cikhulupililo . Iye adzapukuta misozi yonse m’maso mwao , ndipo imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . Ana ena angafunike kuphunzila za Yehova m’zitundu ziŵili — ca kusukulu kwawo ndi cimene amakamba panyumba . Ndipo anthu a m’banja lake amawacitila zinthu zambili kuti awaonetse kuti amawakonda kwambili N’zoonekelatu kuti nkhondo yoyamba ya padziko lonse inayambitsa mavuto amene akhala ovuta kuwathetsa . Popeza kuti nthawi zonse Mulungu amatha kudziŵa pamene nyenyezi iliyonse ili , inunso amakudziŵani bwino panokha . Amadziŵa bwino - bwino pamene muli , mmene mumvelela , ndi zimene mufunikila panthawi iliyonse . ( Aroma 16 : 20 ) Ndiyeno , Mulungu adzalamulila anthu ndi kubwezeletsa cimwemwe ndi mtendele monga mmene anafunila paciyambi . — Ŵelengani Chivumbulutso 21 : 3 - 5 . Anati : “ Zinali monga kuti mtima na maganizo anga zaumbidwanso na kukhala zatsopano . Mwacitsanzo , bwanji ngati wina m’banja lanu kapena mnzanu wapamtima wacita chimo , ndipo wacotsedwa mumpingo cifukwa cosalapa ? M’kupita kwa nthawi , ophunzila Baibulo anaona kuti vinyo weniweni wofiila wosasukuluka ndi umene uyenela kugwilitsilidwa nchito monga cizindikilo ca magazi a Yesu . Conco , kukhala odzicepetsa kudzatiteteza kuti tisawononge umoyo wathu wauzimu . Mfundo imeneyi inaonekela bwino pamene iye anaonetsa Yesu “ maufumu onse a padziko lapansi , ” na kumuuza kuti : “ Ndikupatsani ulamulilo pa maufumu onsewa ndi ulemelelo wawo wonse , cifukwa unapelekedwa kwa ine . Ndikhoza kuupeleka kwa aliyense amene ndakonda kum’patsa . ” Zitsanzo zimene tafotokoza zionetsa mmene anthu a Mulungu akhalila ‘ okhulupilika pa cinthu cacing’ono , ’ kapena kuti cuma cakuthupi , cimene cili na phindu locepa tikaciyelekezela na cuma cauzimu . Usapse mtima kuti ungacite coipa . ” ( Sal . 37 : 8 ) Cifukwa cacikulu cimene tiyenela kupewela ‘ kupsa mtima ’ n’cakuti timafuna kutengela Yehova , amene ‘ saticitila mogwilizana ndi macimo athu . ’ ( Sal . Yesu atamva uthenga umenewu , anauza ophunzila ake kuti Lazaro anali mtulo ndipo anali kufuna kupita kuti akam’dzutse . Koma Yehova ananidalitsa mwa kunithandiza kupeza wophunzila Baibo amene anapita patsogolo mwamsanga . Kumbukilani kuti Mulungu anathandiza Yehosafati ; inunso adzakuthandizani . Tikakhudzidwa na kusintha , kodi uphungu wa Paulo kwa Akhiristu a ku Roma ungatithandize bwanji ? Conco , tiyenela kuuza Mulungu m’pemphelo kuti timafunitsitsa kusinkhasinkha zinthu zimene zimamukondweletsa . Ngati nitakumana na ciyeso cofanana na cimeneci , ningacite ciani ? M’bale Mumba : Anthu ambili amalidziŵa vesili . Anthu mamiliyoni akali mu ukapolo Sangatigwilitse mwala . Cacitatu , mmene Yehova anapelekela cilango kwa Sebina zili na phunzilo lofunika kwa Akhristu amene ali na udindo wopeleka cilango , monga makolo na akulu mu mpingo . Kufuna - funa mwakwama zinthu zimene “ anthu a mitundu ina akufunafuna ” kungawononge cabe unansi wathu ndi Yehova . Nanga n’cifukwa ciani imeneyi ni nkhani yabwino ? Nimakondwela kuona kuti n’nathandiza ana anga kudziŵa Yehova ngati mmene ine nacitila . Abale ndi alongo a mumpingo wina m’dziko la Costa Rica anapindula kwambili ndi makonzedwe amenewa . Iwo analemba kuti : “ Tikayang’ana Nyumba yathu ya Ufumu , timaona ngati tikulota . N’cifukwa ciani m’busa anakonda Msulami ? Iye anati : ‘ N’nali kukwiya nawo kwambili . ’ — Mac . 26 : 11 . Paulo atabatizika , anasintha kwambili khalidwe lake . Koma mbili yake yoipa inali isanathe . Buku la Civumbulutso likufotokoza za kubwela kwa Mfumu “ ndi mphamvu ndi ulemelelo waukulu ” kuti iononge adani a Mulungu . Citsanzo ca Nehemiya cionetsa mmene kudzicepetsa kungatithandizile kupewa kudalila nzelu zathu pamene utumiki wathu wasintha , kapena udindo . Kodi ufanana bwanji na mau a m’mipukutu ina imene ilipo kale ? Posonyeza kuti Yehova amateteza mwacikondi , wamasalimo anati : “ Mulungu sanalole kuti munthu aliyense awacitile zacinyengo , koma anadzudzula mafumu cifukwa ca io . ” ( Sal . 16 , 17 . ( a ) Kodi colinga cimodzi ca misonkhano yathu n’ciani ? Kumbukilani kuti odzozedwa atatsala pang’ono kupita kumwamba , Gogi adzaukila anthu a Mulungu . ( Ezek . Makhalidwe ena na zizoloŵezi zina zoipa zimatenga nthawi kuti munthu asinthe . Conco , mudziziledzela mtima . — Aefeso 4 : 23 , 24 Ngakhale n’conco , sicinali copepuka kwa Yefita ndi mwanayo kukwanilitsa zimene analonjeza . Onse anafunikadi kudzimana zinazake . 17 : 26 ) Koma pali zifukwa zina . Mzimu woyela unawathandiza kumvetsa bwino coonadi ca m’Malemba cimene sanali kucimvetsa poyamba . Koma mfundo imeneyi si ya m’Malemba . 26 : 21 ) Koma kuyankha mofatsa nthawi zambili kumabweza mtima pansi . Mfundo za conco , pamodzi na mafunso oyenelela , mungathandize nazo mwana wanu kuyamba ‘ kuganiza bwino , ’ na kukulitsa cikhulupililo mwa Mulungu . — Miy . 3 : 13 ) Kodi kufatsa kumaonetsela motani nzelu yocokela kumwamba ? M’bale Mumba : Kuti otsatila a Yesu apulumuke , Yesu anaona kuti n’kofunika kuti io adziŵe dzina la Mulungu ndi kuligwilitsila nchito . Paulo analangiza Akristuwo kuti : “ Tsopano ndikukudandaulilani abale , m’dzina la Ambuye wathu Yesu Kristu , kuti nonse muzilankhula mogwilizana ndi kuti pasakhale magaŵano pakati panu , koma kuti mukhale ogwilizana pokhala ndi mtima umodzi ndi maganizo amodzi . ” Koma iye amene amasanthula mitima amadziŵa zimene mzimu ukutanthauza , cifukwa umacondelela m’malo mwa oyela mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu . ” Kodi inu ndinu bwenzi laconco ? Apa n’zoonekelatu kuti kupanga malonjezo kwa Mulungu si nkhani yofunika kuitenga mopepuka . Munthu wina ku Belfast , m’dziko la Northern Ireland , anakamba kuti njinga imene analandila ali na zaka 10 kapena 11 , ndiye inali mphatso yabwino koposa . N’zomvetsa cisoni kuti Aisiraeli atangotsala pang’ono kuloŵa m’dzikolo , analephela kulandila coloŵa cao cimene anaciyembekezela kwa nthawi yaitali cifukwa cogonja ku ciyeso . — Num . Caciŵili cimene cingatithandize kuti tisatenge mbali m’ndale , ndi kukhala “ ocenjela ngati njoka koma oona mtima ngati nkhunda . ” Mvelani citsanzo ca masiku ano . Mwacitsanzo , tinene kuti tikuŵelenga naye Chivumbulutso 21 : 4 . Ngakhale atumwi , poyamba sanamvetsetse cifukwa cake Yesu anawasambitsa mapazi . Makaloni na chizi ni cakudya cimene amakonza mwa kuphika makaloni na kuwasakaniza na supu ya chizi . Paulo amatikumbutsa kuti Mulungu ndi “ amene angathe kucita zazikulu kwambili kuposa zonse zimene timapempha kapena kuganiza , malinga ndi mphamvu yake imene ikugwila nchito mwa ife . ” Ndi Amphamvu , ” Sept . Pambuyo pa nchitoyi , m’bale wina anati : “ Sindidzaiŵala cilengezo cakuti tifunika kulengeza Ufumu ndiponso cangu cimene anthu amene anapezeka pa msonkhanowo anaonetsa . ” Kodi iye anafotokoza kuti wokana Kristu ndani ? ( Yohane 3 : 19 ) Baibulo limasimba kuti kale dziko linaonongedwa m’masiku a Nowa , munthu wokhulupilika . Tidzapewa kunamizidwa kuti tikhulupilile nkhani yabodza imene taŵelenga pa Intaneti , ngakhale kuti nkhaniyo ndi yofala kwambili . Nanga bwanji za anthu oipa amene sadzasintha , amene adzapitiliza kucilikiza dongosolo loipali mpaka pamene cisautso cacikulu cidzayamba ? ( b ) Kodi nkhani ya Yosefe imatiphunzitsa ciani za Yehova ? 10 : 34 , 35 . ( Miy . 27 : 10 ) Koma onani zimene Yesu ananena pamene munthu wina wodziona kukhala wolungama anam’funsa kuti : “ Nanga mnzanga amene ndikuyenela kumukonda ndani kwenikweni ? ” Yesaya 45 : 1 : “ Ine Yehova ndalankhula kwa wodzozedwa wanga . 2 : 2 ; Tito 1 : 10 ) Tsatilani malangizo amene anapelekedwa kwa Timoteyo . Tingapindule bwanji ndi zimene Yesu anatiphunzitsa m’fanizo la zofufumitsa ? Njila imeneyi ingaoneke yosafunika kwenikweni , koma ndi yothandiza kwambili . Acibale a Rute anali kukhala ku Mowabu . Ambili amene amayamba utumiki wanthawi zonse sacita zimenezo kuti apeze phindu . Koma amatelo cifukwa afuna kutumikila Yehova ndi ena . Ngati yakho lanu ni inde , simudzagwila mwala . Mwacitsanzo , magazini ya Zion’s Watch Tower ya March 1 , 1902 , inafotokozako umboni wina . Yehova amakonda cilungamo , ndipo sadzalekelela zoipa mpaka kale - kale . Koma mitengo ya maolivi imapilila kwambili ngakhale pamene kuli cilala . Coyamba , ananitumiza ku tawuni yokongola ya Cirencester mumzinda wa Cotswolds . Mofananamo , ifenso tifunika kukonzekela tsopano mwa kukhala ndi makhalidwe amene adzatithandize kudzakhala m’dziko latsopano . ( Ŵelengani Mateyu 23 : 37 , 38 . ) Baibo ni yosiyana na mabuku ambili amene amatha nchito . 79 : 9 . ( Lev . 22 : 32 ) Mau akuti “ Ine ndine Yehova , ” amene amapezeka nthawi zambili m’buku limeneli , amatikumbutsa kuti tifunika kumvela Mulungu . Haneni anakamba kuti , “ kuyambila tsopano anthu azicita nanu nkhondo . ” 14 : 15 ) Yesu sanangouza ophunzila ake kuti akhale m’cikondi cake . Koma anawauzanso kuti “ akhalebe m’cikondi [ cake ] . ” Nayenso anali na mkazi mmodzi , ngakhale kuti kukwatila cipali kunayamba kale - kale anthu atangopanduka kumene mu Edeni . — Gen . Zimene aneneli analosela zinacitikadi . Baibulo limakamba kuti “ munthu amakhala ndi cikhulupililo cifukwa ca zimene wamva . ” Lemba la Aefeso 5 : 17 limatilangiza kuti : “ Pitilizani kuzindikila cifunilo ca Yehova . ” ( 1 Akor . 3 : 18 , 19 ) Ndinatsiliza maphunzilo a ku sekondale ndili ndi zaka 15 , ndipo ndinasankha zoti ndiyambe upainiya mu January 1971 . Makolo anga anavomeleza zimenezo . N’ciani cinacititsa Mose kupandukila Yehova ? Pa ise tekha sitingacotsepo kupanda ungwilo , ucimo , na imfa . Kumeneko mumaceza ndi Akhiristu anzanu amene amakudelani nkhawa , ndipo amafuna kulimbikitsana wina na mnzake . Citsanzo ca Yesu ciyenela kutilimbikitsa kupitiliza kufunafuna anthu m’magawo athu amene ndi acisoni cifukwa ca zinthu zoipa zimene zikucitika m’dziko lino . Atsuko Yehova anali kufuna kuti io azimvela Cilamulo cake . 18 : 11 ) Ndithudi , cuma cakuthupi cidzatha . Conco , musataye mwayi wociseŵenzetsa mwanzelu kuti ‘ mudzipezele mabwenzi ’ kumwamba . ( 2 Petulo 3 : 5 - 7 ) Anthu ankhanza sadzavutitsanso ena . Kodi alendo angapindule bwanji ngati tiwakomela mtima ? Yehova kupyolela mwa mtumwi Petulo , anapeleka mwai kwa Ayuda ndi anthu otembenukila kuciyuda kuti akhale mtundu watsopano , umene ndi mpingo wacikristu . Cosankha cimeneci cingaoneke ngati nkhani yaing’ono . Koma kodi makolo amayembekezela ana awo kuwacitila ciani ? Baibulo limati : “ Panacita bata lalikulu . ” Yehosafati anakhalabe wodzipeleka kwa Mulungu mofanana ndi Asa , atate wake . Pamene anaopsezedwa ndi gulu lankhondo lalikulu la adani , anadalila Mulungu . CIKONDI ndi khalidwe lalikulu la Yehova Mulungu . 8 , 9 . ( a ) Kodi pali mapindu otani ngati makolo amvetsela ana ao popanda kuwadula mau ? Koma iye anakamba kuti ngakhale kuti “ anali wofunitsitsa kupeleka cuma cake ” kuti cithandizile pa nchito yomasulila Ciheberi , kufufuza kwake kukanangopita pacabe . Mfundo za m’Baibo zimatitsimikizila kuti Mulungu amatikonda ndipo amatifunila zabwino . ” Conco , monga olambila oona , aliyense wa ise ayenela kuyesetsa kucilikiza ulamulilo wa Mulungu . Cokondweletsa n’cakuti hosiyo siinanivulaze . Koma limenelo ndilo tsiku limene acibale anga anadziŵa kuti n’nabadwa wogontha . Colinga ca Marilyn cinali kukakhala miyezi yocepa cabe , koma atakhala zaka , iye anayamba kuona kuti zinthu zayamba kusintha m’banja lake . Ŵelengani Yesaya 40 : 28 . Aisiraeli anali kudziŵa kuti Yehova Mulungu wawo ni “ Yehova mmodzi . ” Koma tinadalitsidwa cifukwa ca khama lathu . ” Kenneth , amene tam’chula m’nkhani yoyamba , nayenso amakhulupilila zimenezi . Timaonetsa kuti timafuna kumvela Yehova . Mwacionekele , tingayankhe kuti , “ Kwa Yehova , ” ndipo imeneyi ni yankho yabwino . Pambuyo pa ciukililo , osalungama adzakhala ndi mwai wophunzila malamulo a Mulungu amene adzadziŵika pamene mipukutu yophiphilitsa idzatsegulidwa . Aisiraeli asanaoloke mtsinje wa Yorodano ndi kuloŵa m’dziko la Kanani , Mose anawauza kuti ‘ azikonda mlendo ’ wokhala pakati pao . ( Deut . Onani zimene mungacite kuti muzikonda kuŵelenga Baibo ndi kuti muzikondwela pamene muŵelenga . Koma Pulofesa Emil Schürer , anati : “ Mphamvu zimene khotiyi inapatsidwa zinali na malile cifukwa Aroma anali kucita ciliconse cimene afuna popanda wina kuwaletsa , maka - maka ngati munthu walakwila boma . Iye amafuna kuti “ anthu , kaya akhale a mtundu wotani ” , akapulumuke . Mulungu anapatsa Nowa malangizo amene anapulumutsa anthu . ( Luka 11 : 13 ) Kumbukilani mtumwi Petulo . Anawatsimikizila kuti adzakhala wokhulupilika kwa anthu amene amam’konda na kusunga malamulo ake . Mkhristu aliyense afunika kukhala wofatsa ndi woleza mtima . M’bale Jürgen ndi mkazi wake , Gertrude , akali kutumikila mokhulupilika monga apainiya apadela ku Germany . M’zaka zimenezo , makolo acikhristu sanali kulimbikitsidwa kweni - kweni kuphunzitsa ana awo Baibo . N’cifukwa ciani dzina la Mulungu linalembedwanso pa mavesi ena 6 m’Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso ? Mwacitsanzo , ganizilani mkazi amene anali ndi nthenda yotaya magazi kwa zaka 12 . Ifenso tiyenela kukhala ndi cikhulupililo cakuti Yehova ndi “ Wakumva pemphelo . ” — Yoh . Khalani Wokhulupilika kwa Yehova , Feb . A Zimba : Palibe vuto . Nitapitako , n’napeza kuti waitana mnzake . Kodi iye anali kumvela bwanji ? N’nadziimba mlandu cifukwa colonjeza kuti nidzapita , koma n’naona kuti nifunika kupitabe . ( a ) Tingaphunzile ciani pa citsanzo ca Robert ? M’malo mwake , iwo amakondwela kugwila nchito mwamphamvu kuti apeze zofunikila mu umoyo wawo na kuthandizanso ena . Amacita izi olo kuti nchito imene amagwila siyokhumbilika . Atayenda ulendo wa tsiku limodzi , amuna atatu amenewa anafika mumzinda wa Ikoniyo . Mwacitsanzo , Baibo imakamba kuti Mulungu anatuma mngelo kukatsogolela Filipo mlaliki wacikhristu kuti akathandize nduna ya ku Itiyopiya , imene inali kufuna - funa citsogozo cauzimu . — Machitidwe . 8 : 26 - 31 . Takamba conco cifukwa Yesu akanapanda kuukitsidwa , sembe tonse tilibe ciyembekezo codzaonananso na okondedwa athu amene anamwalila . Yesu anapeleka citsanzo cabwino kwambili pa nkhani yoona zosangalatsa moyenela . Onani zimene Baibulo imaphunzitsa : Pa mpukutuwo panali uthenga waciweluzo , wolembedwa mbali zonse ziŵili . ( Zek . Pa msonkhano wa mu 1957 , panali anyamata 33 sauzande ocokela m’zigawo zosiyanasiyana za ku England , ndi a ku maiko ena 85 . ( b ) N’ciani cidzatithandiza kusankha mwanzelu kuti tipambane polimbana ndi zinthu zofooketsa ndi zosokoneza utumiki wathu ? Mwacitsanzo , cifukwa ca cikondi , Yehova “ wakhazikitsa tsiku limene akufuna kudzaweluza m’cilungamo dziko lapansi kumene kuli anthu , kudzela mwa munthu amene iye wamuika , ” Yesu Kristu . M’zaka ma 100 angapo oyambilila , anthu ambili anali nayo Baibo m’Cigiriki kapena m’Cilatini . 1 - 3 . ( a ) N’ciphunzitso cina citi cimene ciyenela kukhala mbali ya zikhulupililo zathu zofunika ngako ? Mtumwi Paulo . 15 : 19 ) Koma cifukwa cakuti timakhala na umoyo woopa Mulungu , anthu m’dzikoli amadana nase . Ngakhale akadzakalamba sadzapatukamo . ” — Miyambo 22 : 6 . * Komabe , nthawi zambili cimene cimakhala cothandiza kwambili ndi ‘ kulila ndi anthu amene akulila . ’ Tikathandiza wina , timakhala na cimwemwe cacikulu ngati sitiyembekezela winayo kutibwezela . Source : The Metropolitan Hospice of Greater New York Nditatsala pang’ono kuigwila , inataya wailesiyo n’kuthaŵa . Munthu angandicite ciani ? ” Pasanathe miyezi iŵili kucokela pamene Aisiraeli anacoka ku Iguputo , komanso asanafike ngakhale pa Phiri la Sinai , pakati pawo panabuka vuto lalikulu . 4 : 8 ; 1 Pet . Izi zidzam’thandiza kuti azimasuka kupempha thandizo pankhani zofunika zimene zingabuke . VictorVinter N’nafuna kuyamba kulalikila kwambili . Mariya anali kukhala mu mzinda waung’ono wa Nazareti , kutali na Yerusalemu na kacisi wake waulemelelo . Yesu anapeleka “ lamulo latsopano ” la mmene Akristu ayenela kucitila zinthu ndi abale ndi alongo ao . Ngati zimenezi zinali zoona , ganizilani mmene zikanakhudzila umoyo wathu . M’malo mwa nkhondo , padzakhala mtendele . 3 Mulungu Amakonda Anthu Okhulupilika Koma posacedwa , anthu oipa amenewa adzawongewa . ( Miy . Mwacitsanzo , anthu masauzande amabatizidwa caka ciliconse . Iwo afunikilabe kufikapo kuuzimu . ( Yoh . 1 : 46 ) Natanayeli ayenela kuti anali kuudziŵa bwino ulosi wa pa Mika 5 : 2 , koma anaona kuti mzinda wa Nazareti unali wosayenelela kukhala kwawo kwa Mesiya . Aliyense wokhulupilila mwa ine , ngakhale amwalile , adzakhalanso ndi moyo . ” Pambuyo pa msonkhano wokonzekela utumiki , timapita kukauza anthu uthenga wabwino wa Ufumu . Ndinaganiza kuti mwina ‘ ndinali kupemphela molakwika ’ , ngati siconco , ndiye kuti ‘ Mulungu kulibe . ’ Iwo anali acangu ndi odzipeleka pocita cifunilo ca Mulungu . Kodi mtumwi Yohane anaona masomphenya otani ? 5 : 22 ) Baibo sikamba kuti Yehova ali na cikhulupililo kapena kuti afunika kukhala na cikhululupilo . Ngakhale n’telo , nkhanza za mtundu uliwonse zikucitikabe mumzinda umenewo . Ndipo anthu 10 pa anthu 100,000 aliwonse okhala kumeneko , amaphedwa . Iwo anakamba kuti cifukwa anamva za Yehova ndi zonse zimene anacitila anthu ake . Popemphela kwa Mulungu , Davide anati : “ Maso anu anandiona pamene ndinali mluza , ndipo ziwalo zanga zonse zinalembedwa m’buku lanu . . . Koma pa zifukwa zosiyana - siyana ena ambili amaona kuti kukhala na moyo kwamuyaya n’kosamvetsetseka . ( Yohane 2 : 1 - 11 ) Pa zocitika zina , iye anaphunzitsa mfundo zosaiŵalika . — Mateyu 9 : 9 - 13 ; Yohane 12 : 1 - 8 . Asanapeleke uphungu ku mpingo wa ku Efeso , Pegamo , na wa ku Tiyatira , coyamba anaiyamikila mipingoyo . ( Chiv . Izi zimatithandiza kukhala na cikumbumtima coyela ndi kukhala naye pa ubwenzi wabwino . — Yoh . 14 : 6 ; Yak . Kodi ndimakhumudwa ndikapatsidwa uphungu ? Yesu atatsiliza msonkhano wake ndi ndi ophunzila ake patsiku limene anaukitsidwa , anawathandiza kumvetsetsa udindo wao . N’cifukwa ciani Mkhristu akayamba kukhwima mwauzimu amayambanso kuona mfundo za m’Baibo kukhala zofunika kwambili ? Koma anagwilitsila nchito malangizo a m’nkhaniyo cakuti tsopano amasangalala poŵelenga Baibulo . Kodi makolo angathandize bwanji ana awo mwauzimu potumikila mumpingo wa cinenelo cina ? Koma zimene zinacitikazo ni citsanzo ca ciwonongeko cacikulu cimene cidzabwela mtsogolo . Conco , sitiyenela kudelela mphamvu ya moni . Amasorete anakopela Malemba mosamala kwambili N’zosadabwitsa kuti Yehova anawakwiyila kwambili . ( Num . Yesu atayambitsa Mgonelo wa Ambuye , anakhazikitsa pangano ndi ophunzila ake okhulupilika . Pangano limeneli limachedwa pangano la Ufumu . Kodi munalakwitsa cinacake cimene cabweletsa msokonezo kwa imwe kapena kwa anthu ena ? Patapita zaka zinai , Michael anapita ku Russia ndipo anaona kuti abale anali kufunikabe . Kodi iye amaseŵenzetsa ciani pofuna kusoceletsa anthu ? Iyo imatithandiza kudziŵa kuti Mulungu ndi wacikondi . — Ŵelengani Salimo 103 : 7 - 10 . Yehova ndiye anasankha amene ayenela kukhala mutu wa banja . Kodi zimene naŵelenga ningaziseŵenzetse bwanji mu umoyo wanga ? ’ 15 , 16 . ( a ) Kodi Yehova amamvela bwanji tikamaganizila zaciwelewele ? Ngati acibululu amatsutsa coonadi , umoyo wa mtumiki wa Yehova ungakhale wovuta . Kodi mumasankha mabwenzi amene amakonda Yehova ndi mtima wonse ? Kucita upainiya mu 1952 ( Ŵelengani Luka 6 : 27 , 28 , 31 , 35 . ) Iye mokakamizika anapatulidwa . Ndi Satana . Ganizilaninso za mlongo Paula wa zaka 70 ku Canada , amene sakwanitsa kuyenda cifukwa ca matenda a msana . Yehova anali ndi cidalilo cakuti Gidiyoni adzalanditsa Aisiraeli cifukwa anaona zimene iye akanatha kucita . Ndifufuzeni , inu Mulungu , ndi kudziŵa mtima wanga . ” Uziwaŵelenga usana ndi usiku , kuti uonetsetse kuti ukutsatila zonse zolembedwamo . Koma kodi ndi anthu angati amene anaziona panthawiyo ? Mofananamo , Mulungu anaika mwamuna kukhala mutu wa mkazi . Kuti mudziŵe mmene izi zimacitikila , tambani vidiyo yakuti , Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji ? Ophunzila Baibulo amenewa ndi enanso ambili anali otsimikiza mtima kutumikila Yehova mokhulupilika cifukwa comukonda . 31 : 10 . “ Magazi a Yesu Mwana wake akutiyeletsa ku ucimo wonse . ” Panatenga maola ambili kuti mtima wanga ukhazikike . ” Kodi ndimaonetsa cikondi ndi ulemu kwa a m’banja langa ponse paŵili kunyumba ndi pakati pa anthu ena ? — Akol . Ngakhale kuti Rabeka anakhalako zaka pafupifupi 3,900 , n’zotheka kutengela citsanzo cake . Kodi tiyenela kucita ciani tikapatsidwa cilango ndi Yehova ? Monga Mboni zake , timadziŵika kuti timalemekeza dzina la Yehova . Tsopano , Amy anamanga banja ndi Eric , ndipo onse atumikila monga apainiya apadela . Koma kukumbukila kuti Ufumu wa Mulungu ungathe kugonjetsa zopinga zonse , kungatithandize kupilila . ( a ) N’ciani cinacititsa Mkristu wina kukhumudwa ? Koma anacita ciani ? Zaka za ucicepele zimasila mwamsanga . Ngakhale kuti anakumana ndi mavuto oopsa , Yobu sanamusiye Mulungu . Pambuyo pake , iye anakhala Mboni yobatizika ndi mpainiya wanthawi zonse . M’nkhani yaciŵili , tidzakambilana fanizo la Yesu la anamwali 10 ndi kuona mmene lingatithandizile kukhala maso mwakuuzimu masiku ano . Onaninso njila ina imene Yehova amatikokela kwa iye . Kodi tingakonzekele bwanji kudzakhala m’dziko latsopano la Mulungu ? Koma cocitika cimeneci n’cimene cinatsegula mwayi wakuti tiyambe kupeza mabwenzi pakati pa abale a m’delalo . ” Onetsani kuti mukugwilizana ndi cilango ca Yehova . Iye anakula movutika , koma analabadila uthenga wa m’Baibo ndi kudzipeleka kwa Yehova . Nayenso Hilda wa ku Philippines , anafuna kuleka kukoka fodya . Kodi kungakhale kuti Baibo inapangiwa mosiyana na mabuku ena ? Mwacitsanzo , Baibo imati : “ Kuopa Yehova kudzawonjezela masiku . ” Kodi zimene inu mumakhulupilila n’zofunika kwenikweni ? M’nthawi zamakedzana , anthu ambili anali kukhulupilila kuti dziko ni lafulati . Komanso kumatilimbikitsa kugwila nchito yolalikila . Tidziŵa kuti Yehova amafuna kuti tizilemekeza maboma . ( 1 Pet . Kodi zina mwa zida zimene zingalimbitse cikhulupililo ca wacicepele n’ziti ? Zocita ndi zokamba zathu ziyenela kuonetsa kuti tilibe maganizo otelo . Cifukwa cakuti anali ndi cangu pa kulambila koona , anthu a Mulungu m’nthawi zakale anali kupeleka ndalama zokonzela malo olambilila . Izi zinanipatsa mwayi wopitiliza kuthandiza anthu amene analibe mwayi wophunzila za Yehova . ” Iye anati : “ Tikuyamika Mulungu cifukwa ca mphatso yake yaulele , imene sitingathe n’komwe kuifotokoza . ” ( Aroma 6 : 12 ; 7 : 18 - 20 ) Ngati tilimbana na ucimo uliwonse , timaonetsa kuti timayamikiladi cisomo ca Mulungu mwa Khiristu . ( b ) N’cifukwa ciani kukambilana za kudziletsa n’kofunika kwambili ? M’malomwake , anadzionela okha kuti kukana citsogozo ca Yehova kumabweletsa mavuto aakulu . ( Gen . Iye anati : “ ‘ Nalaŵa ndipo naona kuti Yehova ni wabwino . ’ Kufatsa kungatipatse cimwemwe . ( 2 Timoteyo 4 : 5 ) Mau amenewa anagwila nchito kwa Akristu akale , ndipo amagwilanso nchito kwa ife masiku ano . Cikondi cao cikamalimba , kumakhala kosavuta kucita chimo , ndipo kumakhalanso kovuta kuthetsa ubwenzi wao ngakhale amadziŵa kuti zimene akucitazo n’zoipa . — Miy . N’zoona kuti nkhani zina zimafunika cisamalilo ca akulu ndi atumiki othandiza . M’banja mukabuka mavuto aakulu , kaŵili - kaŵili akulu anali kupeleka thandizo . Ngakhale zili conco , alongo ena cikumbumtima cao cingawalole kuvala cakumutu pazocitika ngati zimenezi . Tikamapemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele , timakhala tikupempha Mulungu kuti Mfumu Mesiya pamodzi ndi olamulila anzake abwele kudzathetsa ulamulilo wa anthu ndi kuononga anthu onse amene amatsutsa Ufumuwo . Malipoti aonetsa kuti m’zaka 5 zapitazi , ofalitsa oposa 250,000 pa dziko lonse anayamba upainiya wa nthawi zonse . Izi zacititsa kuti ciŵelengelo ca apainiya a nthawi zonse cionjezeke kupitilila pa 1,100,000 . Ha ! M’malo mwake , Mulungu adzaononga anthu onse “ amene akuwononga dziko lapansi , ” omwe ndi maboma onse a anthu amene akulamulila masiku ano . Ngakhale kuti anali pa mavuto aakulu , Yobu anayamikila malangizo amene Mulungu anam’patsa . Mwa ici , Mulungu mozizwitsa anacititsa kuti ufa na mafuta ake ophikila zisathe , n’colinga cakuti iye na mwana wake asafe na njala . ( 1 Maf . Yehova anatilamula kuti tiziceleza abale na alongo athu ndi kuwapatsako zinthu zofunikila . Nanga ife masiku ano tiphunzilapo ciani pa cikhulupililo cake ? — 1 Samueli 17 : 11 - 14 . Mwacitsanzo , tingaugwilitsile nchito kuphikila cakudya . Tidzakambilananso mmene Yehova amaonetsela kuti amadziŵa anthu ake , ndipo nthawi zina amacita zimenezi m’njila imene iwo sanali kuyembekezela . 6 : 32 , 33 . Ndiyeno m’madzulo , tinali kuliza belu . Lembani zinthu zimene mufunikila Yehova amene amaona mitima , anauza Yesaya kupitilizabe kulengeza cenjezo limeneli ngakhale kuti ena sadzamvela . Nanga cikwati cimeneco cidzacitika liti ? NYIMBO : 38 , 34 Izi zitifikitsa ku mfundo ina yofunika kwambili kuiganizila — colinga ca wopeleka mphatso . Conco , abale anajambula nkhani 92 zosiyanasiyana . ( b ) Tikambilana ciani m’nkhani ino ndiponso yotsatila ? Nanga n’cifukwa ciani Mulungu sanamuteteze ? Ndipo timapemphela kuti adalitse abale athu amene amacita zambili kuposa ife . ( Mat . 10 : 12 ) M’dela limene Yesu na ophunzila ake anali kulalikilamo kaŵili - kaŵili , anthu anali na cizoloŵezi coitanila alendo m’nyumba zawo . Mwacitsanzo , wacicepele wina ataŵelenga nkhani yakuti “ Kodi Mungalimbane Bwanji ndi Zilakolako Zoipa ? ” Ngakhale kuti kuphunzila citundu cimeneci kunali kovuta , Tiffany wapeza madalitso ambili . Wamasalimo Davide anaimba kuti : “ Ine ndasautsika ndipo ndasauka . Yehova amandiwelengela . Kodi mfundo za coonadi zamtengo wapatali zimenezi n’ziti ? Pamene n’nali na zaka 5 , atate anacoka panyumba n’kutisiya tokha ndi amayi . Anacoka ca ku ma 01 : 00hrs . Kodi kucita zimenezi kunali kopepuka ? Mose anali kuwakonda Aisiraeli . Debora analimbikitsa Baraki kuti apulumutse anthu a Mulungu Mwina cingakhale cifukwa cotunthiwa na anzake . Koma kuseŵenzetsa mashini yopulinthila na mapepa , munthu anali kukwanitsa kupulintha mapeji 1,300 tsiku limodzi cabe . Ndiponso , zolembapo zake za pepa ya gumbwa kapena zacikumba zinali zodula maningi . Anali kutanthuza kuti Yehova payekha ndi wacikwane - kwane . Koma ena anakambe kuti : ‘ Zimenezo n’zosavuta kunena , koma n’zovuta kucita . ’ Gulu lathu limatengela citsanzo ca Ezara na Paulo . Limacita zinthu mosamala kwambili pofuna kuonetsetsa kuti zopeleka zikugwilitsidwa nchito moyenela . Komanso , mtumwi Petulo anaukitsa mzimayi wacikhristu Dorika ( Tabita ) . Mtumwi Yohane analemba kuti : “ Pali zinthu zinanso zambili zimene Yesu anacita . Zikanakhala kuti zonse zinalembedwa mwatsatanetsatane , ndikuganiza kuti mipukutu yolembedwayo sikanakwana m’dzikoli . ” ( Yoh . Munthu wina wakale amene anali paubwenzi wolimba ndi Yehova anali Gidiyoni . Iye anafotokoza kuti : “ Tinakonza zakuti tizikonzekela misonkhano na kucita kulambila kwa pabanja ndi ana athu m’cinenelo cathu . Lembali limakamba za nyama za m’sanga , monga mimbulu na mikango , zimene zidzakhala pamodzi mwamtendele na nyama zoŵeta , monga ana a nkhosa ndi a ng’ombe . 8 BAIBO IMASINTHA ANTHU Liu la cinenelo coyambilila ca Baibo limene analimasulila kuti “ dama , ” limaphatikizapo kugonana kwa anthu amene si okwatilana mwalamulo , ndiponso kugonana kwa amuna okha - okha kapena akazi okha - okha . Iye amafuna kuti mabwenzi ake nawonso akhale na moyo wamuyaya Baibo imati : “ Komatu [ Yehova ] sanam’patse colowa ciliconse [ Abulahamu ] mmenemu ayi , ngakhale kadela kocepetsetsa . M’nkhani yokhudza umoyo wake , M’bale Karl Klein , amene anali mu Bungwe Lolamulila anakamba kuti nthawi ina anapatsidwa uphungu ndi M’bale J . Mabaibo ena amakamba kuti Mulungu anatenga Inoki kupita naye kumwamba . Pofuna cabe kupewa mikangano , mkazi angazilemekeza mwamuna wake ngati ali pafupi naye . Tiphunzilanso mmene Mulungu amasinthila mau ake pokambilana ndi anthu mogwilizana ndi zocitika za panthawiyo . Ndipo pikica yolembedwa pa kapeti imeneyo , imayelekezela mmene munda wa Edeni wochulidwa m’Baibo unalili wokongola . Ndinali wozidalila kwambili . Cikhulupililo ndi cikondi n’zimene zinalimbikitsa Mose kutumikila Mulungu mokhulupilika . Makolo ake anazindikila kuti pali cina cake cimene cimudetsa nkhawa . ( Ekisodo 16 : 18 , 31 ) Koma m’kupita kwa nthawi , io anayamba kuganizila zakudya zosiyanasiyana zimene anali kudya ku Iguputo . Ponena zanthawi imene ana sukulu anali kuphunzila za cisanduliko , iye anati : “ Cikumbumtima canga sicinali kundilola kutengamo mbali panthawi yokambilana . Kuganizila kwambili zimenezi kumatilimbikitsa kupitilizabe kukhala mogwilizana ndi dzina lathu . Kuti tikapitilizebe kusangalala ndi zimene timakonda m’dziko latsopano , kodi tidzafunika kuika ciani pa malo oyamba ? Kukanakhala kuti panalibe munthu amene akanatha kucoka mu ukapolo wa zipembedzo zonama , lamulo la Mulungu lakuti , “ tulukani mwa iye anthu anga ” likanakhala lopanda tanthauzo . Mumpingo wacikhiristu woyambilila , munali Ayuda , Agiriki , Aroma ndi anthu a mitundu ina . Ndinali kukhulupilila kuti akufa angavulaze amoyo , komabe ndinali kufuna kudziŵa zimene Baibulo limaphunzitsa . Anali kutiuzanso kuti tingakhale osangalala ngati titsatila mfundo za makhalidwe abwino za m’Baibulo . — Salimo 37 : 10 , 29 ; Yesaya 48 : 17 . 13 Mbili Yanga ​ — Zinthu Zonse N’zotheka kwa Yehova Umu munali m’mwezi wa May , 1910 . Cinanso cimene cingathandize ndi kuganizila zitsanzo za anthu akale olimba mtima . Iwo adzakhala mbali ya Ufumu wa Mesiya . Anthu ambili anasokonezeka maganizo cifukwa ca nkhondo yoyamba ya padziko lonse ndi fuluwenza ya ku Spain . Pasanapite nthawi yaitali , tinayamba kugwilitsila nchito wailesi yathu yochedwa WBBR . Ndipo pulogalamu yoyamba inaulutsidwa pa February 24 , 1924 . N’cifukwa ciani Mose anataya mwayi woloŵa m’Dziko Lolonjezedwa ? Koma kudzipeleka kwa Yehova kumene ndiye kofunika kwambili kwatibweletsela cisangalalo cosatha . 8 , 9 . ( a ) N’ciani cinacititsa kuti Yesu adyetse anthu masauzande ambili mozizwitsa ? Kukhala wozindikila kunathandiza Yesu ‘ kusakwiya msanga . ’ ( Miy . Motelo , pochula mwacindunji “ cophimba , ” Yesaya anati : “ Iye adzameza imfa kwamuyaya ndipo Yehova , Ambuye Wamkulu Koposa , adzapukuta misozi pankhope zonse za anthu . ” Nyimbo imeneyi , imapezeka pa lemba la Ekisodo caputala 15 , ndipo pa vesi 18 pamati : “ Yehova adzalamulila monga mfumu mpaka kale - kale . Mokhudzidwa mtima , io angafunse kuti : “ Kodi Cinyengo cidzatha ? ” Ngakhale m’Baibo , anthu ena amachulidwa ndi nchito zimene anali kugwila . Tinali kuyenda maulendo ataliatali kukalalikila kwa anthu onse amene anali kukhala m’midzi yambili ya m’cigawoco . Aroma sanali kukakamiza anthu a mitundu ina kuleka cipembedzo cawo , pokhapo ngati cipembedzoco cicita zosemphana ndi boma kapena ngati sicicilikiza makhalidwe abwino . M’dziko latsopano , tidzakhala okondwa kuyendela malangizo a Yehova pogwila nchito yokongoletsa dzikoli , kuphunzitsa oukitsidwa , ndi kucita cifunilo ca Yehova . Komanso , nthawi ina , ine na kagulu kathu ka ulaliki tinapita ku lesitilanti kukadya cakudya pa nthawi yopumula . Tili kumeneko , n’nanyamuka kupita ku toileti . 3 : 9 , 10 . Zikanatenga nthawi kuti io ‘ adzaze dziko lapansi ndi kuliyang’anila . ’ ( Ŵelengani 1 Akorinto 13 : 11 ; 14 : 20 . ) Koma m’malo mwake , iwo anangoika cikhulupililo cawo pa ‘ kukwanilitsika kwa malonjezo ’ a Mulungu . Anali ‘ kufunitsitsa malo abwino koposa . ’ Pali pano , mumzinda wa New York muli mipingo 6 ya citundu ca Cirasha . Pakuti adzapatutsa ana ako aamuna kuti asanditsatile ndipo adzatumikila ndithu milungu ina . Pamenepo mkwiyo wa Yehova udzakuyakilani ndipo adzakuonongani ndithu mofulumila . ” — Deut . Nthawi zina tinali kukhala milungu ingapo osatuma kapena kulandila uthenga . A Zulu : M’loto lake Nebukadinezara anaona mtengo umene unakula kwambili mpaka kufika kumwamba . Yesu anati : “ Samalani zimene mukumvazi . ” Izi zingalimbitse cikhulupililo cathu cakuti akufa adzauka olo kuti papita zaka zambili kucokela pamene zimenezi zinakambiwa kapena kulonjezedwa . Zikanakhala kuti makhoti amatsatila mfundo za m’Cilamulo ca Mulungu , milandu yambili ikanakhala ikuweluzidwa mwacilungamo . 4 : 7 ) Komanso , timakonda na kulemekeza olambila anzathu , podziŵa kuti nawonso ni anthu a Yehova . — Aroma 12 : 10 . Baibulo imati : “ Zitatelo , mzimu wa Yehova unayamba kugwila nchito pa Davide kuyambila tsiku limenelo mpaka m’tsogolo . ” — 1 Samueli 16 : 1 , 5 - 11 , 13 . N’cifukwa ciani anawauza kuti acoke ? Mose ayenela kuti anadziona kuti ndi wosayenelela ndipo sangakwanitse . Ndipo ici ndi cifukwa cina cimene tiyenela kutengela citsanzo ca mkazi wokoma mtima ameneyu . Izi zitanthauza kuti vesili lichula zonse zimene zinalembedwa zokhudza umoyo ndi utumiki wa Yesu padziko lapansi . Ca pakati pa zaka za m’ma 1900 , kunapezeka zidutswa zakale kwambili za Baibo ya Septuagint za m’nthawi ya Yesu . Mwina inu mumakhala ndi nthawi kusiyana ndi ena . Maganizo amenewo amacititsa anthu kukoledwa ndi “ cinyengo camphamvu ca ucimo ” — Aheb . ( Yuda 4 ) Akhiristu osakhulupilika amenewa anali kuganiza kuti angacimwe mmene afunila , ndipo Yehova adzapitiliza kuwakhululukila . ( Agal . 6 : 10 ) Cifukwa cocitila cifundo anthu ocokela m’maiko ena , Mboni zambili zimayesetsa kuphunzila citundu cina . ( 1 Akor . Izi zinaonekela bwino kwambili pamene anapatsa uphungu atumwi ake cifukwa coonetsa khalidwe lodzikonda na mzimu wofunitsitsa ulamulilo . — Maliko 9 : 33 - 37 ; Luka 22 : 24 - 27 . Anati : “ N’nali kulila masiku ena mu wiki , tulo osatuona . Ndinali kukonda kukamba kuti , “ Kubwezela ndi kwa Ambuye , koma akuseŵenzetsa ine monga cida cake . ” Yehova amasangalala kugwilitsila nchito anthu odzicepetsa ndi odzipeleka . Kodi Malemba amaonetsa bwanji kuti kupeleka zopeleka ni mbali yofunika kwambili ya kulambila koona ? Ena angatumile anzao nkhani popanda kuona kuti nkhaniyo ndi yoona kapena ai , kapena popanda kuganizila zotsatilapo zake akatuma nkhaniyo . Olo kuti Sauli anakaniwa na Yehova atalamulila kwa zaka ziŵili cabe , analoledwa kupitiliza kulamulila kwa zaka zina 38 , kufikila pamene anafa . — 1 Sam . Koma unjikani cuma canu kumwamba , kumene njenjete kapena dzimbili sizingawononge , ndiponso kumene mbala sizingathyole n’kuba . ” — Mat . Cifukwa ca khama la Mboni zokhala m’madela amene kumafikila othaŵa kwawo , anthu ambili othaŵa kwawo amvela “ mau a ufumu ” kwa nthawi yoyamba . Koma kumadalila kukhulupilika kwathu pa nchitoyi . Tiyeni tione zitsanzo za anthu amene anapeza mapindu ambili atayamba kuŵelenga Baibo . Ngakhale kuti tuakacisi tumenetu tumathandiza anthu kuti asinkhesinkhe ndi kukumbukila okondedwa ao amene anamwalila , nthawi zambili tumaonetsa zikhulupililo ndi miyambo yacipembedzo ya anthu amene amatupanga . ( Yoh . 11 : 48 ) N’cifukwa cake Mkulu wa Ansembe , Kayafa , anali patsogolo popanga ciwembu ca kupha Yesu . — Yoh . Michael anali kufuna kuphunzila zambili ndipo anavomela phunzilo la Baibulo . Tiyeni tiŵelenge Machitidwe 2 : 21 . ( 1 Petulo 1 : 22 ) Mtumwi Paulo , analimbikitsa anchito anzake kuti akhale ndi “ cikondi cocokela mumtima woyela , m’cikumbumtima cabwino , ndiponso m’cikhulupililo copanda cinyengo . ” — 1 Timoteyo 1 : 5 . Kodi uphungu umene Yehova anapatsa Yobu uyenela kuti unam’thandiza bwanji mavuto ake atatha ? Zimenezi zinali zosiyana kwambili ndi umoyo umene ndinazolowela . Conco , tinawapulintila nyimbo za Ufumu ndi kuwapatsa . Koma tikakhala oleza mtima , cimalimba . ( 1 Akor . N’nasiya Zinthu Zina Pofuna Kutsatila Ambuye ( F . Loyamba ni Aheberi 3 : 4 , ndipo lina ni Aroma 12 : 1 . 16 : 10 , 11 ; 17 : 12 ; Mat . 1 : 5 , 6 ) Wotsatila anali Solomo , ndipo nayenso sanali woyamba kubadwa . — 2 Sam . 6 : 5 , 11 - 13 , 17 . Ngati ndife odzicepetsa , tidzapewa kukakamiza wophunzila Baibulo kubatizidwa . Pa anthu 78,000 okhala pa cilumbaci , ndi anthu 7 cabe amene anafa . Tingacite bwino kudzifunsa kuti , ‘ Nikanakhala kuti si ndine Mboni ndipo anthu abwela kudzanilalikila , kodi nikanamvetsela uthenga wa Ufumu ? ’ HUABI YIN , anaphunzila sayansi yokhudza zinthu zosiyana - siyana . Mwacitsanzo , m’malo mokamba kuti , “ Pepani kuti mwakhumudwa , ” mungakambe kuti , “ Pepani kuti zimene nakamba zakukhumudwitsani . ” 15 : 17 ) Conco , musamaope kuceleza ena cifukwa cofunika ngako ni kuwaonetsa cikondi . Kapena mwacita nsanje cifukwa cakuti ndine woolowa manja ? ’ — Mat . 20 : 1 - 15 . Kukumbukila Imfa Ya Yesu — Liti Ndipo Kuti ? Zoonadi , anthu ambili afa cifukwa ca nkhondo , njala , ndi milili . 15 Pitilizani Kukhala Wacangu mu Utumiki Mulungu adzamenya nkhondo ya Aramagedo osati kuti awononge dziko , koma kuti aliteteze kwa anthu amene akuliwononga . — Chivumbulutso 11 : 18 . Nthawi zina , Nani ndi ine tinali kugwa m’matope popita ku misonkhano . Kodi anali kuganiza kuti Msulami anali kufuna kucita ciwelewele ndi m’busayo ? Iyai . Komabe , Yehova wadalitsa khama lake ndi la ena odzipeleka ngati iye . Atabwelela mumpingo , iye anati : “ Ndikali kukumana ndi mavuto ena pa umoyo , koma madalitso a Yehova ndi ambili kuposa mavutowo . ” Ndinali kufunitsitsa kucoka , koma sindikanalemba mau amenewo . 15 : 16 ) Mwacionekele , mau amenewa anawalimbikitsa ngako atumwi . Mwa pemphelo pendani bokosi yakuti “ Zimene Mungacite Kuti Mukhale na Umoyo Wosafuna Zambili , ” ndipo yambani kucitapo kanthu kuti mukwanilitse zimene mwasankha . Kucita zimenezi kudzatilimbikitsa kupitilizabe ‘ kufunafuna Ufumu , ’ osati zinthu zakuthupi . — Luka 12 : 31 . Katswili wina wa Baibulo anati : “ Mkristu aliyense ali ndi udindo ‘ wopita ’ kukalalikila , kaya ndi pafupi kapena kutali . ” — Mateyu 10 : 7 ; Luka 10 : 3 . Mwa ici , tingafunse kuti , ni mfundo ziti zimene tiphunzilapo pa makonzedwe okhala na mizinda yothaŵilako ? Pofotokoza mfundo imeneyi Yesu anati : “ Mukamasunga mau anga nthawi zonse , ndiye kuti ndinudi ophunzila anga . ” — Yoh . 8 : 31 . Zinaikiwa mu 537 B.C.E . , pamene Aisiraeli anabwelela ku Yerusalemu kuti akamangenso kacisi . Pitilizani kuyang’ana m’lamulo langwilo ndipo yesetsani kukhala ndi mzimu wodzimana . Mwamuna wa Sandra anakamba kuti : “ Ngakhale kuti mlongoyu sitinali kumudziŵa bwino , zinthu zimene anaticitila zinatisangalatsa kwambili . Conco , pofuna kulimbikitsa abale ‘ kufutukula mitima yawo , ’ mu October 2013 , Bungwe Lolamulila linavomeleza makonzedwe apadela othandiza abalewo kudziŵana bwino . ( 2 Akor . N’ciani cimatithandiza kukhulupilila zimene olemba Baibulo analemba ? Iye anauza anthu kuti : “ Malo m’dzikoli akadalipo cifukwa tafunafuna Yehova Mulungu wathu . Mphatso ya dipo ndi cimodzi mwa zinthu zabwino kwambili zimene Atate wathu anaticitila . 11 , 12 . ( a ) N’cifukwa ciani kukhala na colinga cabwino covalila umunthu watsopano n’kofunika ? ( 2 ) Kuwaphunzitsa mocokela pansi pa mtima . Cotelo comboco cinatsala pang’ono kusweka . ” ( 1 Pet . 2 : 12 ) Yehova amakondwela akaona kuti anthu ake onse ndi oyela . Ndingathandize bwanji abale athu amene ali m’ndende ? Olambila Yehova padzikoli adzakondwela kosaneneka pamene adzamva mau a Yesu akuti : “ Bwelani , inu amene mwadalitsidwa ndi Atate wanga . Loŵani mu ufumu umene anakonzela inu kucokela pa kukhazikitsidwa kwa dziko . ” — Mat . 3 , 4 . ( a ) Pangano la Cilamulo linayamba liti kugwila nchito ? Ndipo mtundu wa Isiraeli unavomeleza kucita ciani ? 4 : 18 ; 5 : 11 ) Yehova amadziŵa kuti Akristu tonse ndife opanda ungwilo , ndipo zimenezi zingapangitse kuti tizivutika kucita zinthu mogwilizana . Conco , tiyenela kuyesetsa ‘ kukhululukilana ndi mtima wonse . ’ — Aef . Pa cifukwa cimeneci , Yehova anaononga anthu 24,000 . Nthawi zina , tingaone kuti n’zovuta kusankha kaya kuthandiza ena kapena kucita zinthu zodzipindulitsa . Mphatso zina ni zamtengo wapatali cifukwa zimapelekewa kaamba ka cikondi cocokela pansi pamtima , osati cifukwa cakuti ni udindo wake kucita zimenezo . Kodi ndimwe odzicepetsadi cakuti mumalabadila mukapatsidwa malangizo ? Linali dalitso lalikulu kwa Isaki kukhala ndi mkazi wodziŵa nchito , woceleza , ndi wodzicepetsa . Satana anali kuukila mtundu wa Aisiraeli pa cifukwa cina capadela . Popeza Cilamulo ca Mose cinalembedwa m’Ciheberi , Yesu ayenela kuti anali kukamba za kacilembo kaciheberi . 24 : 45 ) Ni umboni uti umene uonetsa kuti Bungwe Lolamulila likukwanilitsa udindo umenewo ? Yesu anasonyeza mfundo yakuti si onse amene amacita cidwi ndi coonadi amene adzakhala kumbali ya Yehova . Yesu anakamba kuti adzapitiliza kucilikiza ophunzila ake mpaka pamene Ufumu wa Mulungu udzacotsapo maboma a anthu . — Ŵelengani Mateyu 24 : 14 ; 28 : 19 , 20 . Kodi ni zocita ziti , kapena mau ati amene amapangitsa aliyense wa inu kudzimva kuti salemekezedwa ? ( 1 Timoteyo 5 : 1 , 2 ) Mwacitsanzo , ngati titacita ciwelewele ndi m’bale kapena mlongo , tingaipitse munthuyo ndi banja lake . 1 , 2 . ( a ) Tidziŵa bwanji kuti aliyense wa ise angakwanitse kuvala umunthu watsopano ? Ngakhale zili conco , ambili sapeza cimwemwe ceni - ceni pa zimene amacita . Conco , Yesu ayenela kuti anakhumudwa kwambili kuona alembi na Afarisi akupotoza Cilamulo ca Atate wake . Ndimakondanso kuphikila odwala cakudya . ” anali kum’kumbutsa za kufunika koika zinthu zauzimu patsogolo mu umoyo wake . ( 1 Sam . 15 : 22 , 23 ) Conco , ngakhale kuti ciyambi ca Sauli cinali cabwino , mapeto ake anali tsoka lomvetsa cisoni . — ( 1 Sam . Iye anali kusonyeza kuti coonadi tingacipeze m’njila zosiyanasiyana . ( Yohane 17 : 17 ) Coonadi cimeneci cimapezeka m’Malemba ouzilidwa ndi Mulungu , Baibulo . Mose anati : “ Kodi Yehova Mulungu wanu akufuna kuti muzicita ciani , koposa kuopa Yehova Mulungu wanu kuti muziyenda m’njila zake zonse , kukonda ndi kutumikila Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse , ndi moyo wanu wonse , kuti muzisunga malamulo a Yehova ndi mfundo zake zimene ndikukupatsani lelo , kuti zinthu zikuyendeleni bwino ? ” ( Deut . N’ciani cingakuthandizeni kuyamikila colowa canu cakuuzimu ? M’kupita kwa nthawi , anayambanso kupezeka pamisonkhano . Iye angaseŵenzetse ciliconse m’dzikoli pofalitsa mabodza ake . ( 1 Yoh . Hava analidziŵa bwino cakuti analiloŵeza pamtima . ( Gen . Conco , anauzako mkulu wofikapo za mtsikanayo . Mdyelekezi safuna kuti anthu azilemekeza ukwati kapena kuti uziyenda bwino . Kenako , anachula makhalidwe 19 oipa amene anthu ali nawo masiku otsiliza ano . Kusamalila bwino thupi lathu Nthawi ina , pamene iye anapempha Yehova kuti amuthandize kudziŵa bwino njila zake , Yehova anamuyankha kuti : “ Ndidzacita izinso zimene wanena , cifukwa ndakukomela mtima ndipo ndikukudziŵa bwino , ndi dzina lako lomwe . ” Nanga bwanji ise Akhiristu masiku ano ? Kuciyambi kwa zaka za m’ma 1900 B.C.E . , Yehova anali ndi anthu ake apadela padziko lapansi . Iye ni waluso pokopa anthu ndi “ cilakolako ca maso . ” ( 1 Yoh . Cinthu cimodzi cimene cingatithandize ndi kumvetsetsa bwinobwino tanthauzo la mafanizo a Yesu olembedwa m’Malemba Oyela . Mungawafunse mwaulemu kuti akufotokozelenkoni zocitika za mu utumiki wawo . Mtima wacifundo . 6 : 18 ; 1 Pet . 8 Kuthandiza Ana a Alendo Ocokela m’Dziko Lina Fotokozani zimene zinacitika kuti Paulo na Sila aikidwe m’ndende ku Filipi . Ndi kuti kumene anailembela ? Yefita , ndi Hana mkazi wa Elikana , onse anali kulambila Mulungu mmodzi . Hana ‘ anapemphela kwa Yehova kwa nthawi yaitali . ’ Yesu anati : “ Lekani kuweluza ena kuti inunso musaweluzidwe , pakuti ciweluzo cimene mukuweluza naco ena inunso mudzaweluzidwa naco . Ndipo muyezo umene mukuyezela ena , ionso adzakuyezelani womwewo . Usiku wonse , Gidiyoni ndi asilikali ake anathamangitsa Amidiyani ndi asilikali amene anali kuwathandiza mpaka kukafika pa mtunda wa makilomita 32 . Tifunika kukhala osamala kuti tisaleke kuona nkhaniyi kukhala yofunika kwambili . Poyankha , Boazi anam’limbikitsa na mau akuti : “ Ndamva zonse zimene wacitila apongozi ako [ Naomi mkazi wamasiye ] . . . M’funseni mmene anzake amaonela nkhaniyo . Yesu pokamba na anthu amene anali kufuna kukhala otsatila ake , anati : “ Ndinu odala pamene anthu akukunyozani ndi kukuzunzani , komanso kukunamizilani zoipa zilizonse cifukwa ca ine . Yehova ndiye anapatsa Kristu mphamvu yocita zozizwitsa . Conco , sitiyenela kukaikila kuti Mulungu Wamphamvuyonse amatha kulamulila mphamvu za cilengedwe mmene akufunila . Conco , kholo lozindikila lingamuikile malamulo n’colinga comuteteza . ( 1 Akor . ( Onani Bokosi lakuti “ Mukamaphunzila Baibulo , Muzidzifunsa Kuti . ” ) 17 : 9 ) Conco , tiyeni tikambilane mmene tingakanizile zopinga zimene zingatilepheletse kumvela mau a Mulungu . Ngati Mulungu amatikonda , n’cifukwa ciani amalola zinthu zoipa kucitika ? Popeza n’zosatheka kumvetsela mau ocokela kumbali ziŵili panthawi imodzi , tiyenela ‘ kudziŵa mau ’ a Yesu ndi kumumvela . Tikamaceleza abale na alongo athu , timawadziŵa bwino kuposa mmene tingawadziŵile m’zocitika zina . Kupewa nkhongole nthawi zambili kumakhala kwanzelu . Ngati mwininyumba wasankha funso , m’baleyo amatsegula kapepalako ndi kukambitsilana zimene Baibulo limanena pankhaniyo . Ndinalibe buku limenelo , koma ndinali kulifuna . Iwo anabwela padziko lapansi na kuvala matupi aumunthu kuti acite zaciwelewele . Izi zinali zosiyana ndi colinga cimene Mulungu anawalengela . — Yuda 6 ; Genesis 6 : 1 - 4 ; 1 Petulo 3 : 19 , 20 . Mapangano amenewa ndi ( 1 ) pangano la Abulahamu , ( 2 ) pangano la Cilamulo , ( 3 ) pangano la Davide , ( 4 ) pangano la wansembe monga Melekizedeki , ( 5 ) pangano latsopano , ndi ( 6 ) pangano la Ufumu . Ngati muona kuti mwayamba kudzikonda , pemphani Yehova kuti akuthandizeni kuongolela maganizo ndi mtima wanu . Komanso zingakhale zopweteka kwa okalamba kuona kuti umoyo wao wasintha ndi kuti sangathenso kucita zinthu paokha . Mabomawo amacepetsako cabe ziphuphu ndi zotsatila zake zoipa . Iye anayamba kuona zinthu mosayenela , ndipo anavutika maganizo kwambili . Koma anasintha maganizo olakwikawo pamene analoŵa m’malo a Mulungu olambilila . ( Sal . Yesu anaonetsa cikondi cake kwa anthu mwa kucita cifunilo ca Mulungu modzipeleka . Wamasalimo analemba kuti : “ [ Yehova ] sadzakhalila kutiimba mlandu nthawi zonse cifukwa ca zolakwa zathu . ” ( Sal . Pambuyo pake mtima utakhala pansi , ndinam’fotokozela kuti ndeu ndi yoipa ndipo ndinam’sonyeza mmene anapwetekela mlongo wake . Nanga n’cifukwa ciani ? Buku la Chivumbulutso limaonetsa kuti odzozedwa ndiponso anthu ena adzagwila nchito yolalikila . Iwo anali kupita ku msonkhano wacigawo , ndipo makolo ake a Milan anali kuyembekezela kukabatizika kumeneko . Ena agwela m’ciyeso cimeneci mwa kulola maganizo ao kuganizila kwambili zinthu zoipa . Iye anali kudziŵa kuyendetsa motoka . Makolo , mungatengele bwanji citsanzo ca Nowa ? Koma kaonedwe kake ka zinthu mu umoyo ndiye kanasintha kwambili . Ndimakondwela kwambili kupezeka pa misonkhano ya maiko kumene timaphunzila zambili za Atate wathu wakumwamba , Yehova , ndi coonadi ca m’Baibulo . Komabe , Akhristu onse okhwima ali ndi makhalidwe ena ofanana amene amaonetsa kuti ndi ofikapo kuuzimu . 6 : 4 ) Anasankha Akhiristu a cidziŵitso kuti apititse patsogolo nchito yolalikila m’magawo atsopano . ( Mac . Kuti timvetse m’gwilizano umene ulipo pakati pa kukhulupilila mwa Yesu ndi kupulumutsidwa ku imfa , tifunika kudziŵa cifukwa cake timafa . Tiyeni tipite kukakwela phili la Yehova . Tipite kunyumba ya Mulungu wa Yakobo . Conco , ngati nthawi zonse timakamba zoona , sitingafunike kucita kulumbila kuti anthu atikhulupilile . Gawo lawo latsopano linali zisumbu za ku Bocas del Toro ku Nyanja ya Caribbean . Anthu ambili okhala m’zisumbuzi ndi a mtundu wa Guaymi , ndipo ndiwo nzika za delali . Mwacitsanzo , ali pafupi kufa pamtengo wozunzikilapo , iye anapeleka udindo wosamalila amai ake amene mwacionekele anali amasiye kwa Yohane wophunzila wake wokondedwa . — Yoh . 19 : 26 , 27 . ( Ŵelengani Deuteronomo 4 : 5 - 8 ; Sal . Araceli : Ndimakonda kulalikila kwa ansembe ndi masisitele amene ndimakumana nao , mwina cifukwa cakuti ndinali sisitele . Kodi zimene ndikufotokoza zimveka ? Zinathandiza Gidiyoni kudziŵa bwino kwambili Yehova ndi kukhala naye pamtendele . TSAMBA 12 • NYIMBO : 64 , 61 Akristu naonso afunika kumvela lamulo lopewa magazi a nyama kapena a munthu . ( Mac . ▪ Mungapambane Polimbana Ndi Satana ( Maliko 14 : 7 ) N’cifukwa ciani pali kusiyana kwakukulu conco pakati pa anthu ? Tikamatelo , tidzakhala pa ubwenzi wolimba kwambili ndi Yehova ndipo ubwenzi umenewo udzatithandiza kupilila ziyeso . 3 : 1 - 7 ) Koma sikuti basi colinga cake cinalephelelatu . N’napempha kuti nikapezekeko , ndipo ofesi ya nthambi ya mu Austria inanifunsa ngati n’nali kufunanso kukaloŵa nawo kilasi ya namba 32 ya Sukulu ya Giliyadi . M’malo mokhala “ anthu odziŵika ndi dzina [ la Yehova ] , ” Akristu ampatuko amenewa acotsa dzina la Mulungu m’ma Baibulo ao ambili . Iwo atengela miyambo yacikunja . Pa utumiki wake wonse , Yesu anali kulemekeza Atate wake . KUFALITSIDWA KWAKE : Mabaibulo pafupifupi 5 biliyoni amafalitsidwa kwambili padziko lapansi kuposa buku lina lililonse N’ciani cingatithandize kuti tikhalebe ndi “ mtendele wa Mulungu ” ? Mu August 1949 , m’dzikolo munali ofalitsa osakwana 10 . Koposa zonse , cikhulupililo canga calimba kwambili . ” Komanso , tiyenela kukumbukila kuti mavesi a Ciheberi oyambilila analibe zizindikilo za m’kalembedwe , monga mitengelo ( koteshoni ) . Kuti tiyamikile kwambili mwai wokhala ndi dzina la Mulungu , tiyenela kuganizila kwambili tanthauzo la dzina lake . 28 : 18 - 20 ) Mwakutelo , Yesu anapatsa ophunzila ake cuma camtengo wapatali , cimene ndi utumiki wacikristu . — 2 Akor . “ Tsopano Yehova Mulungu anatenga munthu uja n’kumuika m’munda wa Edeni kuti aziulima ndi kuusamalila . ” 21 Musakhumudwe ndi Zolakwa za Ena Mfundo zimenezi zingawathandize kumvetsetsa coonadi ca m’Baibo na kudziŵa mmene angaphunzitsileko ena . Ndipo ndimakhulupililanso kuti iye amatipatsa zokhumba zathu . Nkhaniyi ili ndi mfundo zimene zingatithandize kuti tizigwilizana m’banja , mumpingo , ndiponso polalikila Ngati muli m’cikwati , mnzanu wapamtima ndi mwamuna kapena mkazi wanu . Ndi mautumiki otani amene atumiki anthawi zonse amene akutumikila m’maiko ena amacita ? Pamene Yehova kupyolela mwa Yeremiya analengeza kuti adzacita pangano ndi Isiraeli , zimenezi zinaonetsa kuti pangano la Cilamulo silidzagwilanso nchito . Baibulo limati : “ Mapeto adzafika . ” Zoonadi , Mulungu anathandiza Yosefe na Blessing kumasuka mu ukapolo m’njila zosiyana . A Zulu : N’zoona . Koma kodi n’ciani cimene aliyense wa ise angacite kuti alimbitse mgwilizano umenewu ? Tingaonetse zimenezi mwa kutsatila malamulo ake . Tikupemphani kuti muziphunzila Baibo pamwekha kuti mupeze mayankho pa mafunso aya komanso ena . 5 : 8 ; 12 : 2 ) Lomba tiyeni tikambilane mbali zina za utumiki wanthawi zonse zimene zingakuthandizeni kukhala wosangalala kwambili . Makalata amene analembedwa mu Nsanja ya Mlonda imeneyo , aonetsa kuti Ophunzila Baibulo acijelemani anali ofunitsitsa kulalikila uthenga wabwino ngakhale kuti anali asilikali . Apa , colinga ca Satana cofuna kuwagaŵanitsa cinalepheleka . Ndiyeno , Davide anaponya mwalawo ndipo unayenda mwamphamvu kulunjika Goliyati . Kusukulu ndinali kufunsa aphunzitsi mobwelezabweza mafunso awa : “ N’cifukwa ciani Mulungu analenga anthu ? 7 , 8 . ( a ) Kodi Yehova amatsogolela bwanji gulu lake la padziko lapansi ? Panthawi ina , pamene Satana anayesa Yesu , anamuuza kuti asandutse miyala yeniyeni kukhala mkate , ndi kuti amugwadile ndi kum’lambila . Motelo , Mulungu adzapatsa anthu zinthu zofunika kwambili pamene adzayankha mapempho atatu oyambilila a m’pemphelo lacitsanzo . Lomba n’nazindikila kuti Yehova yekha ndiye angan’thandize ‘ kukhalabe woganiza bwino na kukhala maso , ’ kuti nikwanitse kulimbana na zimene zingawononge maganizo anga , mtima wanga , na cikwati canga . ” ( b ) Kodi m’nkhani ino tidzakambilana mfundo zofunika ziti ? Kodi tidzakambilana mafunso ati ? Blessing * anafika ku Europe ali na ciyembekezo coloŵa nchito yokonza tsitsi . Yesu anali wotsimikiza mtima kuti Baibulo ndi Mau a Mulungu ndi kuti amatipatsa malangizo othandiza kwambili . Kodi kudziŵa coonadi ponena za Mulungu kunam’teteza bwanji Nowa ? ( 1 Sam . 16 : 7 ) Mwacitsanzo , kodi timacita bwanji ngati wacinyamata wasankha zosangulutsa zosayenela , kapena pamene acita zinthu mopulupuza ? Njila imeneyi imacepetsako msonkho umene mwiniwake cumaco amapeleka . ndi zida ziti zimene zakhala zikugwilitsidwa nchito polalikila uthenga wabwino wa Ufumu ? Linakamba za loto lina la mfumu lokhudza mtengo waukulu umene unagwetsedwa , kenako unaphukilanso . Kaya ndi mmenemo , sindikumbukila bwinobwino . Iye anacita zinthu modekha ndiponso mwanzelu . N’cifukwa ciani tifunika kuteteza cuma cathu cauzimu ? Anthu ambili amapatula ola limodzi kapena angapo mlungu uliwonse kuti aphunzile Baibulo . Cifukwa ca kusakhulupilika kwao , Aisiraeli sanakhale ufumu wa ansembe . Koma zimenezo sizinacititse Cilamulo kulephela kugwila nchito yake . Anamuona ataimilila m’cigwa modzitukumula , ndipo anali munthu wamaonekedwe woopsa kwambili kuposa munthu aliyense amene Davide anaonapo . Ndinasamuka kuti ndikaonjezele utumiki wanga kwa Yehova , osati kuti ndikazipindulitse . ” Panthawiyo ndinali ndi zaka 20 , ndipo ndinali msilikali . ( Num . 12 : 3 ) Anakulitsa khalidwe la kudzicepetsa , limene linam’thandiza kucita zinthu modekha ndi anthu osiyanasiyana , ndiponso pa nkhani zovuta . ( Eks . Pamene muŵelenga nkhani ina yake m’Baibulo , dziyelekezeleni kuti munaliko . Mungadzifunse mafunso monga akuti : ‘ Kodi ndikanakhala ineyo ndikanacita bwanji ? Kumbukilani kuti pali zinthu zina zimene zingadzutse cisoni ca munthu . Zinthu zimenezi ni monga zocitika zapadela , nyimbo zinazake , masinapu , ngakhale fungo la zinazake , mau , kapena nyengo inayake m’caka . Komabe , analephela kupanga ubwenzi wolimba na Yehova , komanso sanali na mtima wofunitsitsa kum’kondweletsa . Bwanji osacipanga kukhala colinga canu kuti misonkhano ikalibe kuyamba kapena ikatha , muzikambako na munthu amene simum’dziŵa ? ( b ) Kodi Satana angatinyenge bwanji kuti tigone mwa kuuzimu ? Baibulo limakamba kuti Yehova “ anaika akerubi kum’maŵa kwa munda wa Edeniwo . Anaikanso lupanga loyaka moto , limene linali kuzungulila mosalekeza , kuchinga njila yopita ku mtengo wa moyo . ” Sikutinso basi nkhani izingokhala Baibo , cikondi cake pa Mulungu , na ciyembekezo cake ca mtsogolo , ayinso . Kupitila mwa Yeremiya , Yehova anauzilatu Ayuda amene anali kukatengedwa ukapolo kuti anafunika kukavomeleza umoyo watsopano umenewo . Iye anati : “ Zonse zinali zosiyana kwambili ndi zimene ninajaila . ” Akuluwa amakhala ku Australia , Bangladesh , Belgium , Brazil , France , French Guiana , Japan , Korea , Mexico , Namibia , Nigeria , Réunion , Russia , South Africa , ndi ku United States . MABWENZI abwino ni ofunika , ndipo pamafunika khama kuti ubwenzi ukhale wolimba . 13 Akanayanjidwa na Mulungu Yesu sanacite nao mantha , koma anali “ kuwafunsa mafunso . ” Utumiki wa pa Beteli umakhala ndi mavuto ena amene angakulande cimwemwe , mofanana ndi utumiki wina uliwonse . M’malomwake , mwaukali anauza anthuwo kuti : “ Tsopano tamvelani anthu opanduka inu ! Komabe , mwina muona kuti sindinu okonzeka kubatizidwa . ( b ) N’cifukwa ciani akulu ayenela kuphunzitsa abale acinyamata ? Pamenepa , tinganene kuti Paulo anali kukamba kuti “ mtendele wa Mulungu ” ni wosangalatsa kwambili kuposa mmene tingaganizile . Mwacitsanzo , ganizilani za tsiku limene anamasula anthu ake ku Iguputo . ( 1 Mafumu 17 : 4 , 5 , 13 , 14 ) ( 3 ) Eliya analinso wotsimikiza kwambili kuti Yehova adzaukitsa mwana wa mkazi wamasiye . 4 : 16 ; Luka 21 : 24 . Mu 1976 , ine ndi mkazi wanga anatilola kuloŵa m’dziko la Australia . 118 : 25 , 26 ; Mat . 21 : 7 - 9 ) Koma n’cifukwa ciani tikamba kuti Salimo 118 inalosela za ciukililo cimene cinadzacitika patapita zaka zambili ? Pankhani ya zosangulutsa , gulu lathu silichula mafilimu , maseŵela a pavidiyo , mabuku kapena nyimbo zimene tiyenela kupewa . Ngati nafenso tili na utumiki uliwonse , tiyenela kuucengeta bwino . Kodi Bungwe Lolamulila limagwila nchito bwanji ? Ngakhale pambuyo pakuti io abwelela , nchito yabwino imene io ndi anthu ena a Cifulenci anacita inabala zipatso zabwino . Caka cimeneco ciŵelengelo ca ofalitsa Ufumu cinaculuka ndi 10 peresenti . Tisaiŵale kuti mtima wathu ungatisoceletse . Nyenyezi zimenezi zinaikidwa m’milalang’amba mwadongosolo ndipo mlalang’amba uliwonse uli ndi mabiliyoni kapena matililiyoni a nyenyezi ndi mapulaneti ambili . Monga mmene zinalili kwa Doreen , anthu ambili amavutika maganizo ngati munthu amene amakonda akudwala matenda akupha . Paulo anali kulimbikitsa Akhiristu aciheberi kucita zinthu mogwilizana ndi colinga ca Mulungu . Kodi pamene munali mwana munagwapo ? M’gulu la Mulungu , tili na abale na alongo ambili anzelu amene tingayende nawo . Koma ‘ onse adzasandulika , m’kamphindi , m’kuphethila kwa diso , pa kulila kwa lipenga lomaliza . ’ — 1 Akor . Ndipo Yehova Mulungu anacitadi zimenezo . ( Yobu 42 : 12 - 14 ) Mosakayikila , Yobu anali kuyewabe ana ake a poyamba amene anaphedwa na Satana . ( Luka 4 : 43 ) Zonse zimenezi ni zizindikilo za munthu wauzimu . Anthu akucenjezedwa kuti asawononge ngakhale cakudya cimene anali kudya nthawi zonse , monga mafuta a maolivi ndi vinyo . Ngakhale kuti anali kutumikila m’malo otetezeka mwauzimu , analola zilakolako zoipa kuzika mizu m’mitima yawo na kukula . 16 , 17 . ( a ) N’cifukwa ciani Yesu anauza Petulo kuti : “ Pita kumbuyo kwanga , Satana ” ? Mfundo zina pa nkhani yocititsa cidwi imeneyi zinalembedwa mu Nsanja ya Mlonda ya September 1 , 2015 , mapeji 12 - 15 . Kwa inu abale na alongo amene mwadzipeleka , dziŵani kuti Yehova amayamikila kwambili mzimu wanu wodzipeleka , ndipo sadzaiŵala nchito yanu . — Aheb . Nthawi zambili ndi bwino kungokhala cete . M’malo mopeza zifukwa zodzikhululukila pa zimene munakamba kapena kucita , uoneni kukhala mwayi wanu wokulitsa makhalidwe abwino . Wapolisiyo anakwiya ndipo anamuwopseza kuti adzam’mangitsa cifukwa cokhala wa Mboni . Ndipo zimenezo zinacitikadi . Anaonjezelanso kuti : “ Koma ine ndi a m’nyumba yanga , tizitumikila Yehova . ” Iye anakamba kuti tiyenela kupeleka “ zinthu za Kaisara kwa Kaisara , koma za Mulungu , kwa Mulungu . ” Kunena zoona , palibe aliyense amene angaikwanitse nchitoyi mwa nzelu zake . ( Yer . * Lije , amene tamuchula kuciyambi , ndi abale ake , amakumbukila mfundo zolimbitsa cikhulupililo zimene atate awo anawaphunzitsa pamene anali kuthaŵa . Iwo ni acangu kwambili mu ulaliki , oceleza , acifundo , ndipo ali na makhalidwe enanso abwino . Ndife ofunitsitsa kuphunzitsa coonadi anthu amene acititsidwa “ khungu , ” kapena kunamizidwa ndi atsogoleli acipembedzo . Pamene Mose anali wacinyamata anali kukhala m’banja lacifumu la Aiguputo . Panthawiyo , cinali cosavuta kuti Mose ayambe kulakalaka cuma ndi ulamulilo . Carlos anati : “ Titafika mu mpingo watsopano , mlongo wina anatiuza maina a mashopu amene tingagulemo zinthu zochipa . 17 : 25 , 26 ) Iye anathandiza kuti dzinalo liyeletsedwe . Ndipo kusintha kumeneko kwatipindulitsa bwanji ? Kwa zaka zambili , acikulile amene ali pakati pathu aona kusintha kwina kumene kwakongoletsa mbali ya padziko lapansi ya gulu la Yehova . Buku lina limanena kuti kupilila ndi khalidwe limene limatithandiza kukhala ndi ciyembekezo colimba ndiponso kusagonja tikamayesedwa . 14 : 9 ; Chiv . 15 : 3 ) Komabe , mfundo yakuti Yehova ndi Mfumu ndi yosiyana ndi kubwela kwa Ufumu wa Mulungu umene Yesu anatiphunzitsa kupempha . Koma simuyenela kuopa kupanga zosankha . Kumbukilani kuti anthu aŵili oyambilila anakana ulamulilo wa Yehova , ndipo kuyambila nthawiyo , anthu enanso ambili aukana . Muzipemphela musanayambe kuŵelenga . Yehova anawalimbikitsa ndi kuwadalitsa cifukwa cakuti anali kukonda kwambili zinthu zauzimu . 2 , 3 . ( a ) Kodi ena amakuona bwanji kuimba mokweza pamisonkhano ? Palibe maziko enieni a makhalidwe abwino , ndiponso moyo ulibe phindu kweni - kweni . ” Koma panali cinacake cimene cinamudetsa nkhawa . Conco anawafunsa kuti , “ Abale , mwacita zotani kuti muphunzitse ena kukhala oyenelela maudindo mumpingo ? ” Coyamba , mwa kuuza Eliya kuti “ Wandipeza , ” iye anasonyeza kuti sanali kuganizila kuti Mulungu akumuona . Pali Malemba atatu cabe amene amakamba za Inoki . Ngati munthu wina watipatsa cinthu ca mtengo wapatali , timaiyamikila ngako mphatso imeneyo cifukwa ca zimene anatailapo . Tonse timaona kuti ni dalitso kukhala mu mpingo wacikhristu . Yehova anakambilatu za mgwilizano umenewu . Kodi mavuto adzathadi ? Kazuhiro anafotokoza kuti : “ Patapita mwezi umodzi , mnzanga wina amene anali kutumikila ku Myanmar anamvela za vuto langa . Ndipo mlongo waciyela na amene ananithandiza moleza mtima kupanga masinthidwe amenewo . Iye wakupatsani udindo wocita zimenezo . ( Salimo 51 : 4 , 10 ; 86 : 2 ) M’nkhani ino , tikambilana citsanzo ca Davide ndi ena amene anakhalako m’nthawi yake . Koma kumbukilani kuti Yakobo anafuna kuti mkanjowo ukhale cizindikilo ca kukoma mtima ndi cikondi . Umaposa Kuganiza Mozama Kulikonse ” Iye anaonjezela kuti : “ M’kupita kwa nthawi ndinapeza mabwenzi abwino amene ndimakonda kwambili . ” Kodi Mumathaŵila kwa Yehova ? Ngakhale mtundu wa cakudya anali kucita kuwasankhila . ( 1 Samueli 9 : 2 ) Cotelo anavula zovalazo ndi kuvala covala ca ubusa cimene anali kuvala nthawi zonse poteteza nkhosa . — 1 Samueli 17 : 38 - 40 . Okwatilana amene amakondana ndi kukonda Yehova ayenela kuthetsa mavuto ao , popeza “ cikondi sicitha . ” — 1 Akor . Akatswili ena a Baibo amakamba kuti Yuda anagwila mau buku lina - lake lochedwa Buku la Inoki . Yehova anapatsa makolo udindo wophunzitsa ana awo coonadi , osati ambuye awo kapena munthu wina aliyense . Nditumizeni . ’ ” Tsiku lina pamene n’nali kuyembekeza sitima kuti niyende ku nchito , munthu wina anabwela kwa ine . Ganizilani tate amene akukambilana ndi mwana wake wazaka 7 . N’cifukwa ciani ena amafunika kupatsidwa ulemu ? Nanga m’nkhani ino tidzaphunzila ciani ? Mmene Gayo Anathandizila Abale Ake , May Iye ayankha kuti , “ Ndiye cakale kwambili kuposa zonsezi , ndipo sanacikonzeko . ” Kodi dzanja lamanja la Kristu lidzacita bwanji “ zinthu zocititsa mantha ” ? Mboni za Yehova zimalalikila n’colinga cotamanda Mulungu ndi kudziŵitsa anthu dzina lake . N’zoonekelatu kuti Satana sanamve cisoni pamene Davide anacita cigololo kapena pamene mneneli Mose analephela kulowa m’Dziko Lolonjezedwa . Baibulo limapeleka mayankho ogwila mtima a mafunso ofunika kwambili Ngati munthuyo afunitsitsa kuphunzila , funsoli lingamucititse kuganizilapo kwambili pankhaniyi . Cifukwa cokhumudwa mungalankhule mau amene angakhumudwitse mnzanu wa mucikwati , ndipo zimenezo zingapangitse kuti mkangano ukule kwambili . ” N’cifukwa ciani n’kwanzelu kupewa nkhongole ? Iwo anagulitsa nyumba yao ndi kusamukila m’nyumba ina yaing’ono . Kodi lidzafika poti silingathe kukonzedwanso ? Koma ngakhale kuti ndinabisala , ndinali kucitabe mantha . ( Luka 16 : 9 ) Kusokonezeka kwa zacuma kumene kukucitika m’masiku otsiliza ano , ndi vuto locepa poyelekezela ndi mavuto aakulu azacuma amene adzacitika padziko lonse posacedwapa . 19 : 38 - 40 ) Nikodemo yekha na amene amachulidwako kuti anathandiza Yosefe . Iye anabweletsa zonukhilitsa mtembo . 12 : 17 ) Nkhondoyo ikali kupitilila cifukwa Satana akufunitsitsa kuononga cikhulupililo ca otsalila odzozedwa ndi a nkhosa zina . Inde , malinga ngati mufuna kucita zimene Baibulo imaphunzitsa . M’kupita kwa nthawi tinacoka pa famuyo cifukwa boma linasiya kuthandiza alimi . Asilikali ovulalawo anali kuwatenga ndi kuthamangila nao m’tumanyumba topangidwa ndi malata mmene anali kucitila opaleshoni . idzafotokoza zinsinsi 12 za mabanja acimwemwe . Kumeneko ‘ timalimbikitsana . ’ 2 : 8 ) Koma nchito zina zimaika umoyo wathu wakuuzimu pangozi kuposa nchito zina . Mwina inu simuyankhapo pamisonkhano ndi kukamba nkhani m’sukulu cifukwa ca manyazi kapena cifukwa coona ngati simungakwanitse . Ndipo anthu 4,800 anapezeka pa nkhani zitatu za m’Baibulo zimene zinakambidwa mumzinda waukulu wa Japan . 1 : 13 ) Iye anali kudziŵa kuti Yehova na Yesu anamuonetsa cifundo cacikulu . Kuwonjezela apo , tidzakhala osangalala ndi okhutila kuti tikupeleka ulemelelo kwa Atate wathu wakumwamba . Kodi zokamba zawo nthawi zambili zimaphatikizapo mijedo kapena nthabwala zotukwana ? ’ Mtumwi Paulo anapeleka yankho kuti : “ Mwa kusamvela kwa munthu mmodziyo , ambili anakhala ocimwa . ” Apo nikamba nkhani ya poyela m’Cibiko pa msonkhano wadela Inu abale acikulile , phunzitsani acinyamata kucita zimene mumacita . Simon anati : “ Zinandithandiza kuona zinthu zofunika kwambili pa umoyo ndi mmene ndingakhalile ndi umoyo wosalila zambili . Izi zinatithandiza kukhulupilila kuti malinga ngati tikhalabe okhulupilika kwa Mulungu na kuika Ufumu wake patsogolo , iye sadzatisiya . Zinanditengela nthawi kuti ndileke kugwilitsila nchito zithumwa za mwai , koma pemphelo linandithandiza . Atate ake a Nowa , a Lameki , amenenso anali munthu woopa Mulungu , anafa kutatsala zaka zisanu kuti Cigumula cicitike . Ngati mwayankha kuti inde , pitilizani kucita zimene mungathe kuti muzisonkhana pamodzi ndi abale anu ngakhale zitakhala zovuta . William akumbukila zimene woyang’anila dela wina anamuuza kuti , “ Muzikondwela ndi utumiki wanu osati malo cabe . ” Zimenezi zathandiza abale ku United States kuti azisonkhana ndi kukambilana Baibulo poyela , ndiponso kuuzako ena zimene amaphunzila . Kodi imwe muli na ciyembekezo canji ponena za kuuka kwa akufa ? Anthu ali na nkhawa ndipo akukumana ndi mavuto ambili . Izi zimatilimbikitsa kuwathandiza mwauzimu . Zimenezi zakhala zikucitika , ndipo ifenso zingaticitikile . ( Chivumbulutso 1 : 1 ) Ena amalimbikitsidwa kwambili akaŵelenga Masalimo , ndipo ena amasangalala kuŵelenga malangizo othandiza a m’buku la Miyambo . Mwezi uliwonse , anthu ambili amabwela pa mashelufu a mawilo a mabuku athu amene amaikidwa pafupi ndi malo amene pamapitila anthu ambili . Tidzakambilana mafunso atatu aya : Kodi colinga ca Mulungu ca poyamba cokhudza dziko lapansi ndi anthu cinali ciani ? NYIMBO : 150 , 32 18 : 4 ) Popeza kuti angelo amatiteteza , sitifunika kuda nkhawa kuti gulu la Yehova lidzagwidwanso ukapolo wauzimu . ( Sal . Cimodzi mwa zigawozo cinali kuchedwa kuti “ Babulo ndi Tsidya Lina la Mtsinje . ” M’kupita kwa nthawi , cigawoci anacigaŵanso m’mbali ziŵili . zosangulutsa ? “ Aliyense wofika kwa Mulungu ayenela kukhulupilila kuti iye alikodi , ndi kuti amapeleka mphoto kwa anthu omufuna - funa ndi mtima wonse . ” — AHEB . ▪ Gwilitsilani Nchito Bwino Lilime Lanu Kudzafika mu 1963 , m’dziko la Kyrgyzstan munali Mboni pafupi - fupi 160 . Ambili a iwo anali ocokela ku Germany , Ukraine , na ku Russia . Tenti ya ubweya wa mbuzi imeneyo inali yojujuka cifukwa ca dzuŵa na mvula . Mosiyana ndi Yehova ndi Yesu , ife ndife opanda ungwilo . ( Ŵelengani 1 Petulo 5 : 6 - 10 . ) Tiphunzilapo ciani pa nkhani ya m’Baibo ya Rehobowamu . 5 : 17 . Kodi inu mumapemphela ? N’cimodzimodzi ndi Akristu ofikapo kuuzimu . 3 : 13 ) Palibe aliyense amene angafune kuphonya mwayi wapadela umenewu . Wosimba ni Edward Bazely Komabe , Adamu ‘ anamvela mau a mkazi [ wake ] . ’ Atafika kumeneko , “ Eliya anatenga covala cake cauneneli n’kucipinda . N’ciani cimene ena amacita kuti athandize apainiya mumpingo wao ? KUKHUTILA KOMANSO KUPATSA Koma Nsanja ya Mlonda sin’nali kuikonda cifukwa coona ngati yovuta kuimvetsetsa . Pamapeto pake , tingaleke kutumikila Yehova ndi kutaya mwai wodzakhala m’dziko latsopano . Yoswa nayenso anapatsiwa nchito yaikulu komanso yovuta yakuti aloŵetse anthu a Mulungu m’Dziko Lolonjezedwa . 3 : 28 ) Yoswa asanayambe kulimbana na adani ake , Yehova anamulimbikitsa na mau akuti : “ Monga ndakulamula kale , ukhale wolimba mtima ndipo ucite zinthu mwamphamvu . 5 : 5 ; Yak . 1 : 21 ) Koposa zonse , makhalidwe amenewa amatithandiza kulemekeza Yehova ndi kuthandiza ena kumvela malangizo a m’Baibo . — Agal . Malinga na buku yakuti Mapping Paradise , cifukwa n’cakuti “ akatswili a zacipembedzo . . . alibe cidwi cofuna kudziŵa malo kumene paradaiso anali . ” Anawo anathandiza atate ao kumanga cingalawa , kenako onse analowamo . ( Gen . “ Mau a Mulungu Wathu Adzakhala Mpaka Kalekale , ” Sept . Pamene Yehova analanga Manase , iye anadzicepetsa ndipo anapempha Yehova kuti amuthandize . Iye angatifotokozele bwinobwino za Mulungu wosaonekayo . BUKU la Zekariya limafotokoza masomphenya ocititsa cidwi kwambili . Mwacitsanzo , limakamba za mpukutu wouluka , mkazi wovininkhilidwa m’ciwiya copimila , ndi akazi aŵili ouluka na mapiko ooneka ngati a dokowe . ( Zek . kudziŵa nthawi yabwino yokamba zinthu ? Anawanena kuti anali munthu wa mantha ndi wothaŵa usilikali . Iye anawayang’ana pamaso n’kukamba kuti , “ Nimenye iwe cimunthu camantha ! ” VUTO : Ngakhale zinthu m’dziko zitakhala kuti zikuyenda bwino ndiponso anthu akulandila maphunzilo abwino kwambili , ena angasankhe kucita zinthu mosakhulupilika . Koma mofanana ndi zoumba zakale zogomoka - gomoka , mabuku ambili anaonongeka m’kupita kwa nthawi . Kodi Baibo ya Wycliffe inawakhudza bwanji anthu ? “ Inde Ndipita ” 12 Kodi pali zinthu zolimbikitsa zimene zinacitikila aliyense wa inu mu utumiki ca posacedwapa ? Yesu anakamba kuti anthu amene “ adzaona Mulungu ” afunika kukhala “ oyela mtima . ” Tingaonetsenso ulemu mwa kupewa kucita zinthu mopitilila malile . Monga mmene anacitila nthawi zakale , Mulungu adzapulumutsa anthu ake . Mungatenge buku limeneli pa www.jw.org Panthawi yovuta imeneyo ya cisautso cacikulu , angelo a Yehova wa makamu adzateteza anthu a Mulungu ndi kuwononga amene amatsutsa ulamulilo wake . ( 2 Ates . Kacilembo kocepa kwambili mu alifabeti ya Ciheberi ni י ( yod ) . Aka ni kacilembo koyambilila pa zilembo zinayi zoimila dzina la Mulungu lopatulika lakuti Yehova . ( Aroma 8 : 16 , 17 ) “ Nkhosa ” ndi “ mbuzi ” zikuimila anthu a mitundu yonse , amene sanadzozedwe ndi mzimu woyela . ( Salimo 73 : 3 - 5 , 12 , 13 ) Masiku ano , anthu ambili amacita zinthu zopanda cilungamo , ndipo nthawi zina amene amacita zimenezi ndi atsogoleli amene amati ndi atumiki a Mulungu . 8 “ Musaiŵale Kuceleza Alendo ” ( Luka 9 : 10 - 17 ) Ndipo zakudya zokwana madengu 12 zinatsalapo . M’caka ca 29 C.E . , Yohane Mbatizi anayamba kulalikila kuti “ Ufumu wakumwamba wayandikila . ” ( Mat . Ndiye cifukwa cake , tiyenela kusamala kwambili posankha zinthu zoti tiŵelenge . ( Yak . 2 : 8 , 9 ) Koma mosiyana ndi zimenezi , kukhala na cikondi kudzatithandiza kupewa kukondela anthu ena cifukwa ca mtundu wawo , maphunzilo , udindo , kapena cifukwa cakuti ni olemela . Musataye mtima ngati nthawi zina ulaliki sunayende bwino . ( 2 Tim . Komiti Yoona za Nchito Yofalitsa Mabuku Kodi tingawathandize bwanji anthu ocokela ku maiko ena kukhala omasuka mumpingo mwathu ? Ndipo ananiuza kuti : “ Ulalikile mbali ija ya mseu , ine nidzalalikila mbali iyi . ” Kodi Yesu anacita zimenezi mokakamizika ? Mofanana ndi mzinda wa Uri , mizindayo inalibe maziko olimba cifukwa cakuti inali kulamulidwa ndi anthu osaopa Mulungu . 30 : 9 ) Pambuyo pa Armagedo , Mulungu adzapeleka dziko latsopano kwa anthu amene anali kugwila nchito ndi iye monga mmene anawalonjezela . Edgar Cayce ndi Jeane Dixon analosela molondola zimene zinacitika m’zaka za m’ma 1900 . ( Ŵelengani 1 Akorinto 9 : 19 - 23 . ) ‘ Tivala ciani ? ’ ” Tiyeni tikambilane zambili zokhuza umoyo wa Danieli pa nthawiyo . Conco , kodi kusamba kwa Aroni kumaimila kuyeletsedwa kwa Yesu ? Muzikhala wokonzeka kucitila cifundo ena , ndipo musamafulumile kukwiya . — Mlal . Izi zitacitika , Mulungu anafunika kucitapo kanthu ndithu . Koma anali kufuna kumuthandiza kuzindikila kucepa kwake poyelekezela ndi Mulungu , amene ni wamkulu kwambili . Lembali limati : “ Wolungama adzakondwela mwa Yehova ndipo adzathaŵila kwa iye . ” Ndipo lomba , ndili ndi anzanga kuzungulila dziko lapansi . Iye analangiza otsatila ake kupemphela kuti : “ Ufumu wanu ubwele . Mneneli wokalamba Danieli anali kupemphela katatu tsiku lililonse ndi kuphunzila Mau a Mulungu . ( Dan . Mukatelo , mudzakhala ‘ wofunitsitsa ndi mtima wanu wonse ’ kuthandiza pa nchitoyi kuti dzina la Yehova lilemekezedwe . N’ndani yekha amene Mulungu amam’gwilitsila nchito kutithandiza kumvetsetsa Mau Ake ? Mwina Mose anakumbukila mmene Yehova anatetezela Abulahamu , Yosefe ndi iye mwini pamene anali pansi pa ulamulilo wa mafumu ena aciiguputo . ( Gen . Kaganizidwe kameneka n’kosiyana na malangizo a Paulo akuti tiyenela ‘ kulolelana m’cikondi . ’ Ndipo tidzakambilananso zimene banja ndi mpingo uyenela kucita ponena za okalamba athu okondedwa . “ MUSANDITAYE ” ( b ) Kodi buku la Macitidwe lionetsa bwanji kuti Akhristu ambili oyambilila anapitiliza kuonetsa cikondi ? 2 : 1 , 2 . Kwa zaka zambili , anthu akhala akukhulupilila zosiyana - siyana pankhani imeneyi . ( 1 Sam . 8 : 7 , 9 , 22 ) Komabe , Samueli sanacite nsanje ndi munthu amene anali kudzamulowa mmalo . MANOWA ndi mkazi wake anali kuganiza kuti sangakhale ndi ana . Yesu anakamba kuti ngati tikonda anthu ena koposa iye , ndiye kuti sindife oyenela iye . Kugwila nchito yolalikila kunali kosavuta kwa Akristu cifukwa Ayuda anali kukhala m’madela ambili amene anali kulamulidwa ndi Aroma . Kuti tilimbane ndi zilakolako zoipa , tifunika ‘ kucita pangano ndi maso athu ’ ngati mmene anacitila Yobu . Ife tonse 7 tinali kukumana pamodzi kuti tiphunzile Baibo ngakhale kuti zimenezi zinali zoletsedwa . Ndipo muyenelanso ‘ kudziunjikila ’ cuma cosatha osati cakanthawi . Ndiponso , ‘ mtima wathu wonyenga ’ ungatilepheletse kutsatila malangizo a Yehova . ( Yer . Komanso , pokamba naye , onetsani kuti mukuzindikila kuti pangakhale zinthu zina zimene simunacite bwino zimene zinayambitsa vutolo . Iye anati : “ Nditaona covala camtengo wapatali ca ku Sinara , pakati pa katundu wotsalayo , cokongola m’maonekedwe , komanso masekeli a siliva 200 , ndi mtanda umodzi wa golide wolemela masekeli 50 , ndinazikhumba zinthuzo , ndipo ndinazitenga . ” 3 : 1 ) Zoona , zinthu n’zovuta masiku ano cifukwa anthu ambili ali pa ulova , zinthu n’zodula , cakudya n’cocepa , ndipo anthu ambili ni osauka . 15 , 16 . ( a ) Kodi Elisa anasonyeza bwanji ulemu kwa mphunzitsi wake ? M’malomwake , Yehova afuna kuti tiziganizila zinthu zoyela ndiponso zabwino . Mosakaikila iye amakhala katswili cifukwa cocita zinthu mosiyana ndi anzake . Rosie anakamba kuti , mau awa a Yesu anam’thandiza kusadela nkhawa zimene zingacitike mailo . Zinthu zodetsa zingaphatikizepo zizoloŵezi zoipa monga kukoka fodya kapena kukamba nthabwala zotukwana . ( 2 Akor . Ŵelengani Maliko 4 : 26 - 29 . Mwana wathu woyamba anabadwa patapita zaka zitatu . Ndiyeno n’nayambanso kuganizila cinthu cofunika kwambili paumoyo wanga . Dziŵani kuti palibe munthu wina amene angakupangileni mbili yabwino . Fotokozani kugwilizana kumene kulipo pakati pa moyo wa mtsogolo ndi mmene tiyenela kukhalila masiku ano . Yelekezani kuti mwapita kukaceza kudziko lacilendo kwa nthawi yoyamba . Ganizilani za mmene cipatso ca mzimu cingakuthandizileni . Kodi tiphunzila ciani m’nkhani ino ? Ngati kulambila kwa Pabanja kumacititsa ulesi , mwina n’cifukwa ca mmene mumatsogozela . Ngati mumapewa kudzikonda ndipo mumacita khama potumikila Yehova ndi ena , mumaphunzitsa ana anu kukhala odzicepetsa Alain amene wakhala akuphunzila Ciperisiya kwa zaka 8 anati : “ Ngati nikonzekela misonkhano m’Ciperisiya nimangoika maganizo pa cinenelo . Koma kodi mungacite ciani ngati munalapa ndipo Mulungu anakukhululukilani chimo lanu , koma cikumbumtima canu cikali kukuvutitsani ? ( Tito 1 : 16 ) Tizikumbukila kuti m’nthawi ya atumwi , Akristu oona anali kudedwa ndi anthu ambili . Mwina n’cifukwa cakuti mumagwila nchito kwa maola ambili , mumakhala ndi zocita zambili , kapena mumakhala olema . Patapita nthawi , n’naloŵa m’gulu la asilikali a United States , ndipo ananitumiza ku Germany . Pa Chivumbulutso 21 : 2 , mkwatibwi akuyelekezeledwa ndi mzinda umene ndi Yerusalemu Watsopano . Magulu aciwawa omenyela ufulu wodzilamulila aculuka , mikangano ya zandale ikukulila - kulila , komanso m’maiko ambili , anthu amazonda kwambili alendo ocokela ku maiko ena . Pa Sondo mu wiki imene n’naleka kuchova lottery , namba yanga ya “ mwayi ” inawina . N’zosadabwitsa kuti paradaiso wa padziko lapansi amasonyezedwa m’zinthu zambili za cikhalidwe ca Aperisiya . Ndipo pamene anali m’ndende , Paulo analemba makalata ambili olimbikitsa . Yesu ananena kuti : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” — Mat . Ngakhale kuti sanali kudziŵa kulemba na kuŵelenga , anali kugwilitsila nchito mpata uliwonse kuuzako ena zimene anali kukhulupilila . Apainiya ambili anayamikila zimenezo cakuti anacoka ku Britain ndi kupita ku maiko ena monga France . Anacita izi ngakhale kuti sanali kudziŵa cinenelo ca kumeneko . Zioneka kuti iwo analidi na zibadwa zosiyana . Mmene Timavulila Umunthu Wakale ndi Kusauvalanso , Aug . Masheya : Mungapeleke ku gulu la Yehova masheya amene muli nao m’kampani kapena kukonza zoti lidzalandile masheyawo mukadzamwalila . Kaya timakhala kuti kapena tikukumana ndi mavuto otani , timasonkhanabe pamodzi kuti tilemekeze Yehova Mulungu ndi Yesu Kristu pa nyengo yabwino koposa ya Cikumbutso . Sungatsimikize kuti zimenezo zacitikadi cifukwa ndi zinthu zopanda cilungamo . Zifotokozanso cifukwa cake kuyamikila cikondi cimene Mulungu wationetsa m’njila zosiyana - siyana , kuyenela kutilimbikitsa kuuzako ena mmene angapindulile ndi kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova . Ophunzila a Yesu okhulupilika 11 , ‘ anakhalabe ndi Yesu m’mayeselo ake . ’ Mboni za Yehova zambili zimene zili ku France zikali ndi ziongo za atate ao akale amene anali kugwila nchito yolalikila ndiponso ya ku migodi mwa khama . Komabe , Yesu anadziŵa kuti iwo angasinthe ngati amvetsela malangizo ake amene anawapatsa mokoma mtima ndiponso ngati akhala odzicepetsa monga iye . Pamene muŵelenga Baibo na zofalitsa zathu , ndiponso kupezeka pa misonkhano yacikhristu , mumamva nkhani zolimbikitsa zofotokoza mmene Mulungu anathandizila Akhristu ena kukhala okhulupilika . Koma n’zomvetsa cisoni kuti okwatilana ambili amasiya kukondana ndipo amalekana . ( 2 Mbiri 14 : 1 , 6 , 9 , 10 ) Kodi Asa anacita ciani ? * — Genesis 37 : 23 - 28 ; 42 : 21 . Tiyeni tione . Tingaonetse kuti ndife “ ocenjela ” mwa kuganizila mavuto amene tingakumane nao mtsogolo . Tingacite ciani kuti tidzakhale na ufulu weni - weni ? 20 Pewani Kutengela Maganizo a Dziko Kwa adani a anthu a Mulungu , nchito ya mboni zimenezo inali ngati yaphedwa , ndipo adani ao anakondwela kwambili . — Chiv . Kwatithandiza kwambili . N’nakhala m’timu ya dziko lathu kucokela mu 1949 mpaka mu 1952 , ndipo n’nakacitako maseŵelawa m’dziko la Cuba , Mexico , ndi Nicaragua . Patapita milungu yoŵelengeka kucokela pamene Francis Ferdinand wa ku Austrian anaphedwa , maiko amphamvu a ku Ulaya anakakamizika kuyamba nkhondo . Tingacite zimenezo mwa kuwauzako mfundo zolimbikitsa za m’Malemba , kuwapempha kuti tiyende nawo mu ulaliki , kapena kuwamvetsela pamene afotokoza mavuto awo . Ngakhale kuti panali citsutso , abale na alongo anapitiliza kulalikila ndi zikwangwani m’miseu molimba mtima . Muyenela kuganizila cifukwa cake mukali mbeta . Miyambo 19 : 3 Iwo ataonekela m’khoti , anaonetsa kuti sanadziŵe kuti anacita mlandu waukulu . Kodi mungaitanile atumiki acinyamata kunyumba kwanu kuti mukhale ndi maceza olimbikitsa ? Anthu oposa 210,000 amene anali pamalopo ndiponso amene anamvetsela kupyolela pa Intaneti , anakondwela kwambili cakuti anaomba m’manja kwa nthawi yaitali . Kuonjezela apo , Baibulo limatiuza mmene Mulungu amaonela anthu amene amagwilitsila nchito mafano polambila . MTUMWI Yohane anatilimbikitsa kuti tiziganizila kwambili za cikondi cacikulu ca Yehova pa ife . Kodi Marita ndi Mariya anapeleka citsanzo cabwino cotani kwa ife ? Koma angelo anaonekela kwa abusa amene anali kuŵeta nkhosa kuchile , kunja kwa Betelehemu . ( Aroma 1 : 11 , 12 ) Ndithudi , olo kuti Paulo anali kulimbikitsa kwambili Akhristu anzake , nayenso nthawi zina anafunika kulimbikitsidwa . — Ŵelengani Aroma 15 : 30 - 32 . Komabe , zimenezi zingatanthauze kuti Mulungu ananamiza Adamu . ▪ Pitilizani Kusinkhasinkha Zinthu za Kuuzimu Iwo anali atangomasulidwa kumene mu ukapolo wa ku Babulo wa zaka 70 . ( Sal . 119 : 23 , 61 ) Iye analola kuti Mau a Mulungu amufike pamtima . — Ŵelengani Salimo 119 : 11 , 46 . Kanayankha kuti , “ N’zoona kuti nikasankha koini ya golide nizakhala na ndalama zambili kuŵilikiza kaŵili ndi yasiliva . ( Agal . 5 : 22 , 23 ) Popeza kuti mtendele weni - weni ni cipatso ca mzimu wa Mulungu , tifunika kulola mzimu woyela kutitsogolela kuti tikhale na mtendele umenewu . Amai anakamba kuti zikanakhala bwino ndikanakhala cigawenga kuposa kukhala wa Mboni za Yehova . Yesu anati : “ Limbani mtima . Anthu ambili amakopeka na maganizo a dziko amenewa cifukwa amaona kuti kukhala m’cipembedzo n’kosakondweletsa ndipo n’kopanda phindu . Aliyense amene wabwela nimamumvetsela bwino - bwino , ndipo nthawi zina nimawauza kuti : “ ‘ Mulungu amakonda munthu wopeleka mokondwela . ’ 6 : 9 , 10 . Koma Yehova alibe tsankho , ndipo posapita nthawi itali abale a mitundu yosiyana anayamba kucitila zinthu pamodzi mogwilizana m’mipingo . Pamene ndinali wacinyamata , ndinaphunzilako pang’ono coonadi ndi Mboni za Yehova . MIYAMBO 17 : 22 24 : 3 ) Conco , fanizo limeneli likukwanilitsidwa masiku ano , ndipo lili mbali ya cizindikilo ca kukhalapo kwa Yesu ndi kuti akulamulila monga Mfumu . Mwacitsanzo , olo kuti Davide sanali mwana woyamba wa Jese , Mesiya anabadwa kupitila mu mzela wa Davide . — w17.12 , mape . 24 : 22 ) Monga mmene taonela , mu 66 C.E . cisautso ca ku Yerusalemu ‘ cinafupikitsidwa . ’ YESU anakambilatu kuti otsatila ake adzakolola zokolola zoculuka m’nthawi ya mapeto ino . Yesu anamuyankha kuti : “ Ufumu wanga suli mbali ya dziko lino . ” Takamba zimenezi cifukwa m’munda wa Edeni , Satana anakamba kuti anthufe sitiyenela kuuzidwa zocita ndi Mulungu , koma tiyenela kucita zimene tifuna . Ine ndidzatulutsa mtundu waukulu mwa iwe . Ndidzakudalitsa ndi kukudza dzina lako , ndipo iwe ukhale dalitso kwa ena . Matica anauza Birgit kuti cinali cokondweletsa ndi conyaditsa kuphunzitsa ana a Mboni pa sukuluyo . Kwa zaka zambili , tapindula kwambili cifukwa cogwilizana ndi abale okhulupilika . Mungakonzekele yankho ya funso imeneyi mwa kuŵelenga nkhani yakuti , “ Kodi Niyenela Kukhulupilila za Cisanduliko — Evolution ? ” Kodi cimeneci ni “ cikondi ” ca bwanji ? Iye ndi Bwenzi lathu limene ndi lokonzeka nthawi zonse kumvetsela zokamba zathu . 8 : 4 ) Mlongo wina wa kudela lomwelo anati : “ Ana a sukulu amanyadila kwambili akangodziŵika ndi aphunzitsi ao . Mwamuna wina wofunitsitsa kudziŵa coonadi ca m’Baibo , wabwela kudzamvetsela nkhani yapoyela imene inalengezedwa m’nyuzipepala ya The Irish Times . Nkhani yoyamba idzafotokoza njila zisanu zimene zingathandize cikwati kukhala colimba ndi cokhalitsa , ndiponso cimene cingathandize okwatilanawo kuti asalekane . ( a ) Kodi Yehova anapatsa ndani udindo wolela ana ? Pewani kukhala monga dilaiva wa basi amene sadela nkhawa zonyamula anthu , koma amangodela nkhawa zofika pa sitesheni ya basi iliyonse pa nthawi yake . ( b ) Nanga cinacitika m’caka cimeneco n’ciani ? Ndipo pakhala umboni wotani wotsimikizila zimenezo ? ( Ŵelengani Miyambo 29 : 21 . ) Angelo okhulupilika a Mulungu ayenela kuti anakhumudwa , kukwiya , na kunyansidwa naye kwambili Mdyelekezi . Mpingo woyambawo ni umene ine n’nali kusonkhanamo , ndipo unayamba kuchedwa Upper Bronx . Ngakhale n’conco , sitidzipatula pa anzathu . “ Amene ayesedwa oyenelela . . . kudzaukitsidwa kwa akufa . ” ( Maliko 9 : 33 - 37 ; 10 : 37 , 41 - 45 ; Luka 22 : 24 - 27 ) Pamene Yesu anaukitsidwa , atumwiwo analandila mzimu wa Mulungu ndipo analeka kukangana za amene anali wamkulu pakati pawo . Ndimaphunzila mwamsanga ndikasonyezedwa mocitila cinacake , conco nkhani zimenezi zandithandiza kwambili . ” Ofufuza apeza kuti anthu amene amathandiza ena , zoŵaŵa m’thupi lawo ndi nkhawa zimacepako . Izi zinathandiza kuti Dziko Lolonjezedwa lisadetsedwe , cifukwa Yehova analamula kuti : ‘ Musadetse dziko limene mukukhalamo , cifukwa [ kukhetsa ] magazi [ a munthu ] ndiko kumadetsa dziko . ’ — Num . Bwanji osaphunzilako moni m’citundu cawo ? Ekisodo caputa 2 - 20 , 24 , 32 - 34 ; Numeri caputa 11 - 17 , 20 - 21 , 27 , 31 ; Deuteronomo caputa 34 Kenako m’caka cimeneco , nkhondo yoyamba ya padziko lonse inayamba ndipo ulosi wa m’Baibo unakwanilitsidwa . ( Sal . 130 : 3 ) Tinakumananso na ciyeso cacikulu cotumikila pamodzi ndi akazitape a boma , amene anayamba kugwilizana ndi mpingo mwaciphamaso . Njila ina imene ungakhalile na cidziŵitso n’kukhalako na mapulojekiti osankha nkhani kapena buku imene ufuna kuiphunzila mwapadela . Kucita zimenezi kunandipatsa mwai wodziŵa bwino zimene zili mu mtima mwao . Ufumu wa Mulungu udzayamba kulamulila dziko lonse m’dziko la tsopano . Kucokela pamene Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse inasila , anthu apitiliza kumenya nkhondo padziko . 2 : 22 ) Anzake a kusukulu nthawi zambili anali kumufunsa ngati akali namwali . Kodi ndi katswili wa zandale uti amene akanalosela ndendende zocitikazi ? Panthawi imene Aisiraeli anali akapolo ku Iguputo , io anaculuka kwambili . Utumiki wanga wa upainiya n’nauyambila ku Quetta , kumene kunali kukhala gulu lina la asilikali a Britain . Patapita pafupi - fupi miyezi itatu , asilikali aciroma opitilila 30,000 otsogoleledwa na Cestius Gallus , anayenda ku Yerusalemu kuti akakhaulitse Ayuda opandukawo . Anali wofunitsitsa kucita zambili mu utumiki wa Yehova cakuti anafunsila utumiki wa pa Beteli , ndipo anaitanidwa mu 1971 . Ndimaona kuti ubale wanga ndi Yehova n’cinthu cofunika kwambili . Komabe , pali pano tingaphunzile cinthu cina cofunika ngako pa citsanzo cake . ( 1 Akorinto 15 : 26 ) Conco , m’pomveka ndipo n’cibadwa kusafuna kuganizila za imfa ya munthu amene timakonda . Matendawa amaopsa kwambili akakhudza manja ndi miyendo cifukwa zimenezi zimacititsa kuti ziwalozo zisamagwile nchito ndipo khosi limauma . Kevin wakhala akutumikila monga mkulu kwa zaka 20 tsopano . Mika 7 : 7 KUYAMBILA kale , atumiki a Mulungu akhala akugwilitsila nchito malo apadela polambila Yehova . Zinadziŵika kuti Yehova ndiye Wamphamvuyonse . Iyo inali cabe mafano osalankhula , ndipo inafunika kunyamulidwa kupita kulikonse . Mulungu ananenelatu zimenezi pamene anati : “ Ndidzapatsa mitundu ya anthu cilankhulo coyela kuti onse aziitanila pa dzina la Yehova ndi kum’tumikila mogwilizana . ” Rahabi nayenso anaona dzanja la Yehova . Mwa njila imeneyi banja lingakonzekele ‘ mavuto ndi zopweteka ’ zimene zimabwela ndi ukalamba . 26 : 1 , 2 . Mwacitsanzo , ŵelengani ndi kusinkhasinkha mau a Yesu akuti “ lekani kudziunjikila cuma padziko lapansi . ” Ndipo nkhani zina zimene tinali kuphunzila ndi miyambo ya Tora ndi cinenelo ca Ciheberi . Baibulo limaonetsa kuti Nebukadinezara anacita misala kwa zaka 7 . ( Aheb . 10 : 24 , 25 ) Imatilangizanso kuti tizikhala ogwilizana pa ciphunzitso . ( 1 Akor . Davide anagwilitsila nchito gulaye kuti aphe cimphona cochedwa Goliyati . 3 : 15 ) Satana sanafune kuti Aisiraeli azilambila Mulungu , ndipo kaŵilikaŵili anali kuwasonkhezela kucita macimo . M’malomwake , Uziya “ anakwiya kwambili , ” ndipo ananyalanyaza cenjezo lao . Lamulo limeneli munalibe m’Cilamulo ca Mose . — Mateyu 22 : 39 ; 1 Yohane 3 : 16 . Woyang’anila watsopanoyo anamvetsela mokoma mtima ndi kukambilana naye malemba olimbikitsa . Tifunikanso kukumbukila mfundo yaciŵili yofunika kwambili yakuti , Yehova angaonetse kuti amatidziŵa mwa kuticitila zinthu zimene sitinali kuyembekezela . M’maiko olemela , anthu amalakalaka kukhala na zovala zambili zapamwamba , nyumba ikulu , kapena galimoto yodula . Tingaone bwanji dzanja la Mulungu pa umoyo wathu ? N’taseŵenza pafupi - fupi kwa mwezi umodzi m’fakitale yokonzela mabuku , n’naikidwa m’Dipatimenti ya Magazini cifukwa n’nali kudziŵa kutaipa . M’nkhani ino , tikambilana za mwambo wapadela kwambili wa cikwati ca mfumu umene watenga zaka pafupi - fupi 2,000 kukonzekela . 103 : 14 ) Cifukwa copanda ungwilo , tingacite colakwa mobweleza - bweleza . Kapena ganizilani mmene zinthu zikanayendela ngati munthu wa m’nkhani imene mwaŵelengayo akanacita zinthu mosiyanako . — Deut . ( Aheb . 12 : 6 ) Ifenso tingaonetse kuti tikuyenda m’cikondi mwa kupeleka uphungu kwa ena pakakhala pofunikila kutelo . ( Miy . N’zoona kuti mavuto ena a m’banja simungawapewe , koma sikuti mungalephele kuwathetsa . Citsanzo ca Naboti cimatiphunzitsa mfundo yofunika kwambili ( Onani ndime 11 ) NDINABADWA m’caka ca 1955 ku Queensland m’dziko la Australia . * — Aroma 7 : 24 . Tsopano ndidziŵa kuti Yehova amasangalala kwambili ndi utumiki wanga kuposa pamene ndinali kupenyelela zamalisece . Posacedwapa , mkulu wina anamufunsa cifukwa cake anatenga nthawi yaitali asanapemphe kubwezeletsedwa mumpingo . Kodi mukufunitsitsa kucita ciani ? N’zoonekelatu kuti ndi Mboni za Yehova zokha zimene zikulalikila uthenga wabwino padziko lonse , ndipo uthenga umenewu umapeleka ulemelelo ndi citamando kwa Yehova . — Salimo 34 : 1 ; 51 : 15 . Ayuda ena pofuna kunyoza Yesu , anakamba kuti iye ni Msamariya . Ciŵelu cina madzulo , apo nili na zaka 5 , ine na atate tinali kugaŵila Nsanja ya Mlonda ndi Consolation ( imene tsopano imachedwa Galamukani ! ) 21 : 1 - 4 ) * Anthu onse amene adzapulumuka padziko lapansi adzasangalala ndi zinthu zambili zabwino zimene Mulungu adzapeleka cifukwa ca cikondi cake . Pambuyo poyenda mtunda wa makilomita 150 kupita ku Beere - seba , analoŵa m’cipululu . Christine na Gideon 1 : 28 ) Koma io sanayamikile zinthu zabwino zimene anapatsidwa . Mu 1947 , dziko la India linagaŵidwa paŵili . ( 1 Mafumu 21 : 18 ) Kodi Ahabu analakwa ciani ? Kumbukilani kuti nawonso , Mulungu wathu wacikondi anawapatsa ufulu wodzisankhila njila imene afuna kuyendamo . — Yes . Pambuyo pake , “ mzimuwo unamulimbikitsa kupita kucipululu . ” Yesu anali “ wofatsa . ” ( Mat . Zinthu monga zimenezo zingatipangitse kukhala bize cakuti tingakhale na nthawi yocepa kapena kukhala tilimbiletu nthawi yoganizila zimene Mulungu amafuna kuti ticite . Kukambilana pasadakhale komanso momasuka kumathandiza acibanja kuika maganizo awo pa kusamalila wodwalayo . Taona ! Mkulu wa manesi anabwela ndi kundilanda bukulo . Iye anali atatsimikiza mtima kucita zimenezo , ndipo kuganizila zimenezo kunamulimbikitsa kukwanilitsa colinga cake . ( 1 Sam . Tinafuna kuyamba kucita bizinesi , koma Atate anauza mlongosi wanga kuti , “ Ngati ufuna , ungapite kukacita upainiya , ndipo izi tidzazileka . ” Iye ananyamula moto ndi mpeni wophela nyama , ndipo iwo anapitila limodzi . ” ( Eks . 34 : 14 ) N’ciani cinam’thandiza Danieli kutsatila malamulo onse aŵiliwa mokhulupilika ? Pelekani zitsanzo . Cifukwa cakuti anaonetsa makhalidwe aŵili awa:kukonzeka ndi kukhala maso . Kodi ndinu okonzeka kugwilitsila nchito njila zatsopano zolalikilila m’gawo lanu ? Kuyambila nthawi imeneyo , anthu ambili a ku Europe ndi a m’maiko ena anayamba kumasulila ndi kufalitsa Mabaibo kuti ngakhale anthu wamba apindule na Mau a Mulungu . Timakumana ndi mavuto monga ulova , matenda , cizunzo , masoka a zacilengedwe , kubeledwa katundu , ndi mavuto ena . Tiyenela kufufuza m’Baibulo ndi m’zofalitsa zathu kuti tipeze mau abwino amene tingakambe . 33 : 1 - 3 . 8 : 41 - 43 ) Mofananamo , masiku ano anthu amene si Aisiraeli a kuuzimu afunika kugwilizana ndi anthu a Yehova , amene ndi “ ana a Ufumu , ” kapena kuti Mboni za Yehova zodzozedwa . Nthawi zina , tingakumane ndi mavuto cifukwa ca kudzipeleka kwathu , koma tikamvela Yehova , iye amatidalitsa kwambili . Mofanana ndi ciwombankhanga cimene ‘ cimaona kutali kwambili , ’ Yehova nayenso amatha kuona zimene zidzacitika m’tsogolo kwambili . Mbali yoyamba , kodi acikulile angathandize bwanji acinyamata kutenga maudindo aakulu ? Ndipo n’cifukwa ciani zimenezi n’zofunikila ? ( 2 Tim . Yehova watipatsa Baibulo kuti lizitilimbikitsa . 25 : 8 - 18 ) Pambuyo pake Davide anauza Abigayeli kuti : “ Adalitsike Yehova Mulungu wa Isiraeli , amene wakutumiza kudzakumana nane lelo . ” Nanga n’ciani cingatithandize kuonabe zinthu moyenela tikakumana ndi mavuto ? Koma ife timafuna kucita zinthu zokondweletsa Yehova . Mtumwi Paulo anauzilidwa kulemba za khalidwe la Isimaeli kuti kunali kuzunza . 145 : 16 . Mlal . Uthenga wabwino wa Ufumu wa Mesiya ndi nkhani imene imatisangalatsa . Malinga n’zimene zili pa Yesaya 32 : 1 , 2 , kodi akulu ali na udindo wanji ? Ngati sitisamala ifenso tingatengele mtima wodzikonda umene wafala m’dzikoli . — Aef . Akhiristu a m’zaka 100 zoyambilila anadziŵa kuti bungwe lolamulila linali kutsogoleledwa ndi Yehova Mulungu kupitila mwa Mtsogoleli wawo , Yesu . Yehova amakukondani ndiponso amakuonani kuti ndinu amtengo wapatali . Paulo sanafotokoze zonse zimene “ maziko olimba a Mulungu ” anali kuimila . Poopela kuti adzafa ndi njala m’cipululu , io anayamba kung’ung’udza kuti : “ Tinali kudya mkate ndi kukhuta ” mu Iguputo . — Ekisodo 16 : 1 - 3 . Iye ndi wamphamvu , wankhanza , ndi wacinyengo . Pofuna kudziŵa zakutsogolo , olosela ena anali kuseŵenzetsa matumbo a zinyama ndi a anthu komanso kuona mmene tambala adobela zakudya . Yehova afuna kuti tidziŵe kuti amatikonda , ndi kuti sayang’anitsitsa pa zolakwa zathu . 1 : 4 ) Conco , kusangalala komanso kunyadila ndi zimene tacita kapena zimene ena acita n’kwabwino . Usaope kapena kucita mantha cifukwa Yehova . . . ali ndi iwe . ” — 1 MBIRI 28 : 20 . Mmene Mungalangile Ana Anu — July - August 10 : 9 - 48 ) Panthawiyo gawo lolalikila linakhala dziko lonse lapansi . Posapita nthawi , mtsikanayu akubatizika . Kwa zaka zambili , atsogoleli acipembedzo sanali kufuna kuti anthu aziŵelenga Baibulo . Iwo anali kuzunza aliyense amene anali kupeza akuŵelenga Baibulo , ndipo anapha anthu ena amene anali kulimasulila . Komabe , Akhristu a m’zaka 100 zoyambilila sanali kucita mwambo wacipembedzo umenewu wa kukhala wosakwatila . 16 , 17 . ( a ) Tingacite ciani kuti tidziŵane bwino na anthu ocokela ku maiko ena ? Kristu , amene amachedwanso “ mngelo wa phompho , ” adzapambana pa nkhondo yolimbana ndi adani ake pamene adzaponya Satana ndi ziŵanda zake kuphompho . ( Chiv . Kaya mukumana ndi mavuto a bwanji , kodi simungakondwele kukhala ndi mnzanu amene mungamauzeko nkhawa zanu ndiponso amene angakuthandizeni ? Ngati ndife oona mtima , tidzakhala ndi cikumbumtima coyela pamene tikambilana ndi anthu mu ulaliki Ndiyeno ananyengelela Adamu kuti nayenso adye . ( Gen . M’Baibulo timaŵelenga za anthu ena amene anali kudwala ndipo anafuna kudziŵa ngati adzacila . ( Mateyu 22 : 39 ) Ndipo Mulungu angathe kudziŵa kuti munthu ali ndi maganizo abwino kapena ai cifukwa iye amaona za mumtima . — 1 Samueli 16 : 7 . Baibulo limatiuza kuti mapeto adzaphatikizapo cionongeko . Ilo limati : “ Pa nthawiyo kudzakhala cisautso cacikulu cimene sicinacitikepo kucokela pa ciyambi ca dziko mpaka tsopano . . . ( 1 Atesalonika 4 : 9 , 10 ) Mwacitsanzo , kodi pali Phunzilo la Nsanja ya Mlonda limene linakulimbikitsani kuonjezela utumiki wanu , kuongolela mapemphelo anu , kapena kuyesetsa kukhululukila abale ndi alongo anu ? 11 : 10 ) Yesu anati : “ Atate wanu Abulahamu anali wosangalala poyembekezela kuona tsiku langa . ” ‘ Mphamvu za kuzindikila ’ : Luso lotha kusiyanitsa cabwino ndi coipa ndiponso lotithandiza kusankha coyenela . Acicepele mu mpingo wacikhristu amapindula ngati aika mtima wawo pa kucita zinthu zokondweletsa Yehova . Kodi Mulungu amafuna kuti olambila ake onse , acinyamata ndi acikulile , azicita ciani ? Iye anatsimikiza mtima kuti sadzadzibisanso kuti ni wophunzila wa Yesu . Ku mbali ina , fuko la Benjamini , limene linali mbadwa za mwana waciŵili wa Rakele , linakhala mbali ya ufumu wa kumwela , pamodzi ndi fuko la Yuda . ( 1 Tim . 5 : 8 ) Yehova amafuna kuti tikhale ndi umoyo wabwino , ndipo timadziŵa zimenezi tikaganizila zinthu zabwino zimene iye anapatsa Adamu ndi Hava . ( Gen . Iwo akuphunzitsidwa kukonda Mulungu ndi anthu anzao , kukhala oyamikila , kusamalila ndi kuteteza cilengedwe , ndiponso kukhala ndi moyo mogwilizana ndi colinga cimene Mlengi analengela anthu ndi dziko lapansi . Pali zambili zimene ana afunika kudziŵa kuposa kungodziŵa cabe malamulo a panyumba , kapena cilango cimene angalandile akalakwitsa . N’zosangalala kudziŵa kuti zozizwitsa zimene Yesu anacita pamene anali padziko zinali kusonyeza zinthu zabwino zimene Mulungu adzacitila anthu mu ulamulilo wa Mesiya . Kodi ukapolo wa ku Babulo unasiyana bwanji na ukapolo wa Aisiraeli ku Iguputo ? Ine na mnzanga wocita naye upainiya , tinali osiyana ngako . Potsiliza , tinafika mumzinda wa Manila pa 19 November , 1954 . Pafupifupi zaka 300 Yesu asanabadwe , akatswili odziŵa Ciyuda anayamba kumasulila Malemba a Ciheberi m’citundu ca Cigiriki . Nditafika zaka 15 , ndinapata mphoto yondilipilila maphunzilo pa sukulu ina yochuka yophunzitsa kuvina ku London yochedwa The Royal Ballet School . Kodi analipo amene akanam’pulumutsa Paulo ? Feb . 12 : 16 - 18 , 26 ) Conco , sitiyenela kucitila nsanje m’bale wathu ngati zinthu zamuyendela bwino , koma tiyenela kukondwela naye . Conco , tikamacita zinthu mogwilizana ndiye kuti tikuphunzila mmene tidzacitila tikadzakumana ndi mavuto mtsogolo . A Daka : Cabwino ndamva . Yehova wapeleka malangizo m’Mau ake amene angatithandize kukhalabe okhulupilika ngati Mkhristu mnzathu watilakwila . — Sal . Patapita zaka , mtumwi Paulo anafotokoza mmene Yesu anapelekela citsanzo ca kulimba mtima pamene “ anapeleka umboni wabwino kwambili pamaso pa Pontiyo Pilato . ” ( 1 Tim . Cifukwa cakuti tikukhala m’dziko la Satana , nthawi zina cikhulupililo cathu cingafooke , tingakhale ndi nkhawa kapena kukhumudwa . Iye anadziŵa kuti Atate ake adzamuthandiza ndi kum’patsa cakudya panthawi yabwino . Iye ndi amene anali kutipatsa malangizo pa nchito yokonza ndi kusunga zipatso ndi ndiwo . Mfumu yatsopano , Yesu , amene akuchedwa Mikayeli , anaponya Satana ndi ziŵanda zake padziko lapansi . Kodi uthenga wofunika umene uli m’fanizoli ndi wotani ? M’kupita kwa nthawi , Mulungu anauza Nowa kuti adzabweletsa cigumula pa dziko lapansi . Kodi Uziya anacita ciani ? Iye anakamba kuti pamene ‘ anthu anali m’tulo , ’ Mdyelekezi anafesa namsongole m’munda umene Mwana wa munthu anafesamo tiligu . ( Aef . 4 : 32 ) Mwakutelo , mumapewa zocitika zobweletsa nkhawa . 6 , 7 . ( a ) Kodi ‘ kukonda Mulungu ’ kumalimbikitsa bwanji Akhristu kuthandiza abale awo ovutika ? Ndipo anacita zimenezo cifukwa anaona kuti khalidwe langa lidzanibwetsela mavuto . Kodi Yesu anacita bwanji na khalidwe la tsankho ? Kodi anali na mbali pa msonkhano wa mkati mwa wiki ? Kodi anapilila ciyeso ca cikhulupililo cake kapena analalikila ku sukulu ? Popeza ndise opanda ungwilo ndipo tikukhala m’dziko lolamulidwa na Satana , tidzapitilizabe kukumana ndi mavuto . ( 1 Yoh . Iye anasonkhanitsa “ ana a Ufumu ” kukhala gulu la anthu , pokwanilitsa ulosi wa Yesaya wakuti : “ Kodi dziko limatulutsidwa ndi zoŵaŵa za pobeleka tsiku limodzi lokha ? Mwacitsanzo , Mfumu Sauli anafuna kupha Davide , anthu ena anafuna kumuponya miyala , ndipo ngakhale mkazi wake anamuseka . Conco inu makolo , coyamba muzicita khama inu eni kuphunzila Baibulo na zofalitsa zathu . 14 : 19 ; 17 : 1 , 4 , 5 , 13 ) Kodi mzimu wotsutsa wa Ayuda unamukhudza bwanji Paulo ? ( Man and Microbes ) Nthomba , malungo ndi TB ndi ena mwa matenda opatsilana amene apha anthu mamiliyoni ambili - mbili m’zaka za m’ma 1900 . [ Zithunzi papeji 6 ] [ Eni Zithunzi ] Ganizilani za kusintha kumene Bungwe Lolamulila linapanga posacedwa . Kodi Yehova anaonetsa bwanji kuti anali kumvetsetsa mavuto ake ? Kuti tipite patsogolo na kukhala munthu wauzimu , tifunika kudzipenda moona mtima . “ Mofanana ndi zimenezi , Atate wanga wakumwamba sakufuna kuti mmodzi wa tianati akawonongeke . ” — Mateyu 18 : 12 - 14 . Nthawi zina , tingaone kuti siticita zambili mu utumiki wa Mulungu kapena tingakaikile ngati Yehova amakhutila na zimene timacita . Koma afunikanso kukumbukila kuti ali na udindo waukulu kwambili . ( Yak . Ngakhale n’conco , mwai ukalipo wakuti anthu azidzipeleka kugwila nchito m’madipatimenti ena pamisonkhano . Tiyeni tikambilane zinthu 6 zimene Paulo anakamba . ( Amosi 8 : 11 ) Iye analonjeza kuti odzozedwa adzakhala “ ngati mame ocokela kwa Yehova , ” pamene akulengeza uthenga wabwino wa Ufumu mothandizidwa ndi a “ nkhosa zina . ” Titangofika na kuwoloka pa buliji , bulijiyo inaphulitsidwa . Nkhaniyo inali kukamba za civomezi capamadzi cimene cinacitika ku Sumatra mu 2004 , cimene cinalengetsa zigumula zamadzi zoopsa m’mbili yonse ya anthu . Kazuhiro anakhala na nkhawa . ( Aroma 15 : 33 ) Tidzasangalala ndi madalitso amenewa pokhapo ngati tithetsa mikangano mwamtendele . Palibe nchito iliyonse imene ingandipatse cimwemwe cofanana ndi cimene ndimakhala naco pothandiza anthu kuphunzila za uthenga wabwino m’cinenelo cao . ” ( 1 ) Kodi aliyense wa ise angakonzekele bwanji kuti akapindule pa Cikumbutso ? Kodi pakhala zotsatilapo zotani cifukwa ca maphunzilo amenewa ? Panthawi yonse imene atumwi analipo na moyo , iwo anali kusamalila bwino mpingo wa Mulungu . Ndiye ganizilani mmene Yehova ndi mmene anthu ambili amaseŵenzetsela molakwika mphatso yawo ya ufulu wosankha zocita , ngakhale kuvulazila anthu ena . 7 : 23 ) Masiku ano , munthu aliyense padziko lapansi ndi mbadwa ya Nowa , ana ake ndi akazi ao . ( Levitiko 25 : 23 - 28 ) Naboti sanafune kucita zinthu zosemphana ndi Lamulo la Mulungu . Kuti mapemphelo athu akhale ovomelezeka kwa Mulungu , tiyenela kuyesetsa kucita zinthu mogwilizana ndi zofuna zake . Mu mpingo wanu wakale , munali wozika “ mizu , ” titelo kukamba kwake , cifukwa munali na mabwenzi abwino ndiponso munali na cizolowezi cabwino cocita zinthu zauzimu . Wokhala pampandoyo , anali wooneka ngati mwala wa yasipi , ndi mwala wofiila wamtengo wapatali . Utawaleza wooneka ngati mwala wa emalodi unazungulila mpando wacifumuwo . ” — Chivumbulutso 4 : 2 , 3 . Kodi kucedwa kubatizika kumacititsa munthu kusakhala na mlandu pa maso pa Yehova akacimwa ? Maganizo aconco angapangitse kuti tiyambenso kufuna - funa zinthu za m’dzikoli , zimene tinaziona kale kuti ‘ n’zacibwanabwana ndi zosathandiza . ’ Zidzakhala zokondweletsa kwambili kuonana ndi Inoki . Kodi cilango ca Yehova cimaonetsa bwanji kuti amatikonda ? Iye anati , “ A Doris anali kucita bwino kwambili , ndipo sindinafune kuwasokoneza . Popeza tili chelu , kodi ndife otsimikiza mtima za ciani ? ( 3 ) Kugwilitsila nchito mafanizo oyenelela . Amatipatsa cikondi cake . NYIMBO : 15 , 74 Charles Harris , amene anakhala mpainiya kwa zaka zambili anafotokoza kuti mavuto amene anakumana nawo polalikila kumadela akutali anam’cititsa kuyandikila kwambili kwa Yehova . Wolemba nkhani wina anati : “ M’caka ca 1914 , dziko linali kuoneka kuti zinthu mtsogolo zidzakhala bwino kwambili . ” Cifukwa tinalengedwa kuti ‘ tiziopa Mulungu woona ndi kusunga malamulo ake cifukwa zimenezi ndiye zimene munthu ayenela kucita . ’ ( Mlal . Ndipo mudzapeza nthawi yoyamikila Yehova pa zinthu zabwino zimene watiphunzitsa . N’CIANI cimene azimai amacita posankha zipatso zoti agule pamsika ? Yosefe anazindikila kuti abale ake amamuzonda kwambili . Kodi zipembedzo zimene sizifuna kuchula dzina la Mulungu zingasiyane bwanji ndi mabungwe ena onse othandiza anthu ? Kodi timaonetsa cikondi kwa ena m’njila yapadela iti ? Akanileni ngati apempha zinthu zosayenela . Pa cifukwa cimeneci , abale anayamba kuchulana maina awo eni - eni oyamba monga akuti José kapena Paulo , m’malo mwa ziwongo zawo . Kodi mitundu iŵili imeneyi ya ma IUD imaseŵenza bwanji ? Paulo anachula makhalidwe monga kudzicepetsa , kufatsa , kuleza mtima , ndi cikondi . Ngakhale kuti cifuno cake cakuti anthu a m’chechi asinthe ndi kudziŵa coonadi sicinakwanilitsike , zimene Lefèvre anacita n’zosaiŵalika . Iye anathandiza anthu wamba kudziŵa Mau a Mulungu . 6 : 18 - 20 . Ndipo kuonjezela pamenepo , mwana woyamba kubadwa wa Mulungu anali ‘ kusangalala ndi zinthu zokhudzana ndi ana a anthu . ’ 20 : 35 ) Umu ni mmene zinthu zimakhalila paumoyo . Koma tisaiŵale mfundo imene tikukambilana . Conco , mufunika kusankha mosamala malemba a mfundo zazikulu , kuŵaŵelenga , kuwafotokoza , kupelekapo fanizo , ndi kumveketsa bwino mmene tingaseŵenzetsele mfundo zake . ( Neh . Baibo imati iye “ anapitiliza kupilila moleza mtima ngati kuti akuona Wosaonekayo . ” ( Yesaya 30 : 19 ) Baibulo limakambanso kuti : “ Koma pemphelo la anthu oongoka mtima limam’sangalatsa . ” — Miyambo 15 : 8 . Dzina lakuti “ Tattannu ” linalembedwa ku mbali imodzi ya colembapo ici cadothi Kukamba zoona , timacita cidwi na mmene Mulungu amalamulilila . 1 : 6 ) Iye adzatipatsa ciliconse cofunikila n’colinga cakuti tisagonje tikakumana ndi ciyeso . Cikumbumtima cathu cimaonetsanso mtundu wa munthu amene tili . Paulo anakamba mfundo imodzi - modziyo , pamene anati : “ Aliyense payekha adzalandila mphoto yake mogwilizana ndi nchito yake . ” ( 1 Akor . “ Aneneli akulosela monama , ndipo ansembe akupondeleza anthu ndi mphamvu zao . . . . Onani masitepu ofunikila kutenga . Ndiyeno , pofuna kum’thandiza kuti aphunzilepo kanthu , angam’patse cilango casaizi . Azariya anati : “ Yehova akhala nanu inuyo mukapitiliza kukhala naye . Mukamufunafuna iye adzalola kuti mum’peze , koma mukamusiya nayenso adzakusiyani . ” Yehova anauza Eliya kupita kwa Ahabu . Thierry anati : “ Seŵelo litatha , tinayamba kuomba m’manja , ndipo ine n’nayang’ana mkazi wanga na kumufunsa kuti , ‘ Kodi ise tingayende kuti kukatumikila ? ’ Kuyambila ali mwana , iye anali kulalikila uthenga wabwino mwacangu . ( Luka 4 : 5 - 7 ) Mofananamo , Satana amadziŵa kuti Yehova analonjeza kuti adzatipatsa zinthu zambili zabwino m’dziko latsopano . Ndinaphunzila zinthu zambili zokhudza Yehova pamene tinali kutumikila ku Japan , ku Nepal , ndi ku Bangladesh . Pamene anali kuyesa kudzikonza , anamva kugogoda pa citseko . Mu 2007 , m’bale Yury ndi mkazi wake Oksana , a zaka za m’ma 30 ndi mwana wao Aleksey amene ali ndi zaka 13 a kudziko la Ukraine , anapita kukaceza ku ofesi ya nthambi ya ku Russia . Conco , musakambe ciliconse cimene simungafune kukamba iwo ali maso . ” ( Agalatiya 3 : 19 ; Aheberi 10 : 1 - 10 ) Kuonjezela pamenepo , Cilamulo cinateteza mzele wa makolo a Mesiya ndi kuthandiza Aisiraeli kumuzindikila atabwela . Izi zinathandiza kuti tizikwanitsa kucita misonkhano ku Paraguay komanso ku Brazil . Nkhani yokhudza umoyo wa M’bale Klein inafalitsidwa mu Nsanja ya Olonda ya Cilengezi ya October 1 , 1984 . [ Cithunzi papeji 29 ] Kuti mudziŵe zambili pankhani ya mmene moyo unayambila , onani kabuku kakuti Was Life Created ? Ngati zokamba ndi zocita zathu zigwilizana ndi ziphunzitso zimenezo , ndiye kuti tikhoza mayeso ndi kuonetsa kuti tili “ m’cikhulupililo . ” Ganizilani zimene Danieli anacita pamene kunakhazikitsidwa lamulo la boma lakuti kwa masiku 30 , anthu asapemphele kwa mulungu kapena kwa munthu wina aliyense , koma kwa mfumu cabe . ( Aef . 2 : 8 ) Anthu m’paradaiso wathu wauzimu adzapitiliza kuculuka mpaka dziko lonse likadzale na anthu angwilo , acilungamo , ndi acimwemwe kuti dzina la Yehova likatamandike kwamuyaya . Mu 1956 tinayamba kuyendela mipingo monga oyang’anila dela . Potsiliza , Don anaŵelenga Mateyu 9 : 36 . Pambuyo pake anapempha Peter kuti adziŵelengele yekha vesiyo . Ni mavuto anji amene tingakumane nawo mumpingo ? Mose ( Gen . 7 : 11 ) Caciŵili , kumbukilani kuti mosiyana ndi masiku ano , pa nthawiyo kunalibe mpingo wa atumiki a Mulungu amene akanamulimbikitsa Nowa mwauzimu . Mayi wina wabizinesi anakamba kuti kompyuta imene atate ŵake anamupatsa pamene anali pa sukulu , ni mphatso imene inasintha umoyo wake . Pamene tiphunzila za Yehova ndi makhalidwe ake , timayamba kuona dzanja lake ndi ‘ maso a mtima wathu . ’ Kuwonjezela apo , anaphunzila maluso othandiza amene akanapangitsa kuti anthu ena amulembe nchito . Cofunika ni kuŵelenga Mau a Mulungu mwakhama , kusinkha - sinkha zimene taŵelenga , na kulola zimene taphunzilazo kusintha umoyo wathu na kutitsogolela . ▪ Mulungu adziŵa kuti zipembedzo zambili zimamuneneza ndi kunyalanyaza mfundo za m’Baibulo . Conco , iye adzaziononga . — Chivumbulutso 18 : 4 - 9 . Motelo , kupeleka cilango cifukwa caukali kapena cifukwa cokhumudwa , sindiye kulanga . Ndiye cifukwa cake mtumwi Paulo analemba kuti , “ ucimo unaloŵela m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi [ Adamu ] . ” — Aroma 5 : 12 . Ndinali kugwila nchitoyi kwa ola limodzi m’maŵa mulimonse kwa zaka pafupifupi 20 . Conco , tizipewa zovala zimene zingatseke matu a anthu amene tifuna kuwalalikila . Koma zimene ndimadana nazo ndi zimene ndimacita . ” Kodi kuŵelenga na kusinkha - sinkha nkhani za anthu ochulidwa m’Baibo kungatithandize kucita ciani ? Pamene Davide anali kutumikila Sauli , nthawi zambili anali kubwelela kwawo kukaŵeta nkhosa , ndipo nthawi zina anali kukhalako nthawi yaitali . Kodi mumacita zonse zimene mungakwanitse kuti mukhalebe maso mwauzimu ? Pambuyo pake , wadela ananipempha kusamukila ku Arkansas kukathandiza mpingo wa El Dorado . M’caka cimeneci Ophunzila Baibulo anakhala ndi msonkhano wao woyamba m’Cipolishi kudela lochedwa Bruay - en - Artois . Kukamba zoona , Baibulo limaonetsa kuti Mulungu saona anthu osadziŵa cifunilo cake kuti ndi osafunika . Peter ataŵelenga lembali , misozi inalengeza m’maso mwake , ndipo anafunsa kuti : “ Kodi ndine mmodzi wa nkhosa zaconco ? ” Pambuyo poti atumwi afa , mpatuko unafalikila mumipingo yonse . Ngati n’conco , n’ciani cimakucititsani kukhala wacimwemwe ? Komabe , Lily anali kuganizila makhalidwe abwino amene Carol anali nao , moti anamuthandiza kwa zaka zambili mpaka pamene Carol anadwala ndi kumwalila . Timafuna kuyeletsa dzina la Mulungu . Tingayambe kutangwanika ngako na zocitika za paumoyo . Anthu ena a Mulungu anali kukhumudwa akaona kuti Mulungu sayankha mapemphelo ao . Abale amene amakamba nkhani pa misonkhano imeneyi amakhala na mwayi waukulu ngako . M’nkhani yosimba za moyo wake , M’bale Diehl anati : “ M’mwezi wa May 1949 , n’nadziŵitsa ofesi ya nthambi ku Bern kuti nifuna kukwatila . ” kulimbitsidwa ndi mzimu woyela ? Kodi zinangocitika mwangozi ? Kodi Yesu anabadwa pa tsiku liti ? Cifukwa cakuti Alexander Wamkulu anafutukula ufumu wa Girisi mwa kugonjetsa madela ambili . Komabe , Abuda amakhulupilila kuti munthu akabadwanso mobweleza - bweleza , mphamvu ya maganizo ake imafika pa mkhalidwe wochedwa kuti Nirvana . Akafika apo , munthuyo amapeza cimwemwe cacikulu . Makalavaniwo anali kugwilitsidwa nchito ndi apainiya amphamvu amene akanakwanitsa kuthana ndi zovuta ndi kuwakonza akawonongeka . Iwo anayesa - yesa kuti anikope na cikhulupililo cawo , koma poyamba sizinaphule kanthu cifukwa n’nali woloŵelela kwambili m’zamaseŵela . Mau a Mulungu anatsogolela Yesu . 17 : 5 ) Kothela , patangotsala masiku oŵelengeka kuti Yesu aphedwe , Yehova anakambanso naye kucokela kumwamba . — Yoh . 12 : 28 . N’zoona kuti ayenela kugula zovala zimene akonda , koma zikhalenso zoti akavala azimila bwino Yehova Mulungu . Kodi tingalimbitse bwanji mgwilizano pa nchito yolalikila , mumpingo , komanso m’banja ? Zimenezi zinacitika pafupi ndi kacisi wa mulungu wamkazi wochedwa Athena mumzinda wa Atene wakale . Iye anati : “ Ndimakhulupilila kuti munthu afunika kugwila nchito mwamphamvu kuti akhale wacimwemwe . Iye amacitila akazi mwacilungamo ndipo amawalemekeza . Komabe , timalandila nchitozo cifukwa timadziŵa kuti kusintha kumacokela kwa Yehova ndipo kumatipindulitsa . “ Muvale umunthu watsopano . ” — AKOL . Tonse timaonetsa ulemu kwa Mtsogoleli wathu Yesu mwa kumvela ndi kugonjela amuna amene iye akuseŵenzetsa kuti atitsogolele . — Aheb . ( a ) Kodi anthu angaganize ciani pa zimene Yehova anacitila Mfumu Azariya , zimene zinalembedwa pa 2 Mafumu 15 : 1 - 5 ? Atumiki a Mulungu amakono amakhala ndi moyo wosonyeza kuti anadzipeleka kwa iye . 9 , 10 . ( a ) N’ndani angafunike kucelezedwa kwa nthawi yaitali ? N’nayamba kumuona kuti ni Tate wacikondi amene amafunila zabwino ana ake . Tsanzilani Cikhulupililo Cao | Debora Cikhulupililo cimazikika pa zinthu ziŵili zimene sitingaone : ( 1 ) “ zinthu zoyembekezeledwa . ” Izi ziphatikizapo zinthu zimene Mulungu anatilonjeza kuti zidzacitika kutsogolo , koma zikalibe kucitika . Zinthu monga kucotsedwapo kwa zoipa zonse ndi kubwela kwa dziko latsopano . M’bale aseŵenzetsa Baibo kuuzako ena uthenga wa Ufumu kwa amuna aŵili okhala kumidzi m’dela la mapili ku Ethiopia . Ganizilani citsanzo ca Rudolf Graichen , amene anabadwila ku Germany mu 1925 . ( Sal . 65 : 2 , 4 ) Tsopano , tiyeni tione nkhani ya m’Baibulo imene ionetsa mmene Mfumu Asa wa ku Yuda anayandikilila Mulungu , ndi mmene Mulungu anamuyandikilila . Kuti mukhale nalo , mufunika kuŵelama ndi kulitenga . Cifukwa cakuti anayamba kuyang’ana mphepo ndi mafunde . Pambuyo pake , anathandiza kupeka nyimbo yonena za kusakhulupilika kwa anthu ake kuti : “ Anayamba kusankha milungu yatsopano . Atatelo m’pamene nkhondo inafika m’mizinda . ” 1 : 3 ; Tito 2 : 2 . Palibe Munthu Angatumikile Ambuye Aŵili , 4 / 1 Tingapeleke bwanji cilimbikitso cogwila mtima ? ( Mateyu 4 : 8 , 9 ) Yesu anakana , ndipo pambuyo pake ananena kuti Mdyelekezi ndiye “ wolamulila wa dziko . ” Pokonzanso Baibulo limeneli , a m’komiti yomasulila Baibulo anapenda mosamalitsa mafunso masausande ambili ocokela kwa omasulila . 10 : 17 - 19 ) Anthu osankhidwa a Mulungu anayenela kulandila mlendo aliyense mumzinda wao , amene anali wofunitsitsa kumvela malamulo opelekedwa ndi Mose . ( Lev . Popeza kuti pali cidziŵitso cambili - mbili m’dziko lamakono , kodi Baibo ni yakale kwambili cakuti siingatithandize masiku ano ? Atsogoleli acipulotesitanti naonso amacita cimodzimodzi . Sindinali kum’patsa mpata wotsiliza kukamba zimene afuna . Atsogoleli a ku Ulaya analephela kuthetsa mikangano ya maiko kuti nkhondo ya padziko lonse isayambe . Tiyenela kutsatila uphungu wa pa 1 Akorinto 10 : 12 kuti tipewe kudzidalila kwambili . Zimene a Willie anakamba zinawakhumudwitsa amayi , cifukwa anali kudziwa kuti atate wawo anali munthu wabwino . Ngati mkazi satenga pakati , angayambe kukhala na nkhawa kwambili . Lembani bajeti imene mudzakwanitsa kuitsatila * Pamene mbadwa za Abulahamu , Isaki , ndi Yakobo zinaculuka kufika mamiliyoni , Yehova anapanga mtundu wa Isiraeli wakale kucokela ku mbadwa zimenezi . Ndiyeno ndinakumana ndi mnyamata wacichaina amene anali kufufuza zinazake pa yunivesite kudela lathu . N’ciani cathandiza Kyung - sook kupilila ? Iye amadana ndi cisalungamo , ndipo panthawi yake adzacotsapo anthu amene apitiliza kucita zosalungama . ( Amosi 7 : 14 , 15 ) Mofanana ndi Amosi , Yehova ananiyang’ana ine , mwana wa mlimi wosauka wa m’tauni ya Liberty , ku Indiana , na kunikhuthulila madalitso ambili amene siningathe kuwachula onse . Ponena za cifukwa cimene cidzacititsa munthu kuweluzidwa kuti ndi nkhosa , magaziniyo inakamba kuti anthu adzaweluzidwa kuti ndi nkhosa cifukwa cokhulupilila Yesu ndi kukhulupilila kuti Ufumu udzabweletsa zinthu zabwino . Conco , imwe makolo mufunika kumadalila malangizo a Yehova pophunzitsa ana anu . Timaika zinthu za kuuzimu patsogolo ndi kukhala umoyo wosalila zambili n’colinga cogwilitsila nchito nthawi yathu yaikulu pa nchito yolalikila mapeto asanafike . — Mat . Phula linali loculuka m’madela oculidwa m’Baibulo . Tumapepala tonse twatsopano twauthenga tunalembedwa mofanana . Kodi panakhala zotsatilapo zotani ? Anafunikilanso kusiya mzinda umene unali ndi mamaliketi kapena tumashopu togulako zakudya monga cimanga , mpunga , nyama , zipatso , zovala , na zinthu zina . Nov . Kusintha kumeneku kunathandiza anthu a Mulungu akale kucita zinthu mogwilizana ndi cifunilo cake . Koma Sauli atafa , Abineri sanakhale ku mbali ya Davide . Kodi dzina la Yehova limaonetsa ciani ? Nanga Satana ananyozela bwanji dzina lopatulika la Mulungu ? Kuyambila m’nthawi ya atumwi , Akristu ambili akhala akupemphela kuti Ufumuwo ubwele . Komabe , ndalama zimene anasunga zitatha , cimwemwe cawo cinasanduka cisoni . Potsilizila pake tinali kulalikila anthu a pafupi . Ndipo Baibo sionetsa kuti iye anali ndi ana . Kusintha mwanjila imeneyi si kopepuka . Koma n’kotheka cifukwa mzimu wa Mulungu umathandiza anthu amene amafunitsitsa kucita cifunilo cake . Mwacitsanzo , nthawi zambili Satana Mdyelekezi anali kusonkhezela Aisiraeli kucita macimo monga dyela ndiponso ciwelewele . Dayska anati : “ Kukumbukila kuti Yehova ndiye anandipempha kuti ndikatumikile kwina kunandithandiza kuvomela mosavuta . ” Tingadziŵe makhalidwe ake ena mwa kuganizila zinthu zimene anapanga . ( Deuteronomo 31 : 19 , 30 ; 32 : 2 ) Tiyeni tiphunzile zinthu zina zokhudza mame ndi kuona mmene utumiki wathu ulili ngati mame n’colinga cakuti tiziphunzitsa anthu mogwila mtima , “ kaya akhale a mtundu wotani . ” — 1 Timoteyo 2 : 3 , 4 . 11 : 9 ) Ndithudi , Yehova amafuna kuti imwe acicepele muzikhala acimwemwe . Timadziŵa kuti Yehova amatisamalila makamaka pamene atipatsa uphungu . KODI mwamuna ayenela kusamalila bwanji mkazi wake ? Ndipo onse adzatsatila “ m’busa mmodzi . ” Kodi kuyamikila cisomo ca Mulungu kuyenela kutithandiza kucita ciani ? Kodi Yehova adzathetsa bwanji makhalidwe oipa ndi mavuto padziko ? Musangoona kuti malinga amapezeka ku misonkhano , ndi kupita nanu mu ulaliki , ndiye kuti ali na cikhulupililo . ( Chivumbulutso 12 : 12 ) Ndinacita cidwi kuona kuti Mbonizo zinalankhula ndi ine mwamtendele komanso ndi mtima wonse . Analinso wokonda kwambili zinthu zauzimu . Conco cimene Mulungu wacimanga pamodzi , munthu asacilekanitse . ” Nayenso mtumwi Yohane anali mzati mu mpingo wacikhristu woyambilila . ( a ) Kodi Yehova anamucitila ciani Hezekiya ? Iwo analimbikitsidwa ndi lemba la Mlaliki 11 : 4 limene limati : “ Woyang’ana mphepo sadzabzala mbeu , ndipo woyang’ana mitambo sadzakolola . ” N’ciani cidzatithandiza kukhala wofunitsitsa kuthandiza ena ? Yehova watipatsa “ mphatso yake yaulele , imene sitingathe n’komwe kuifotokoza . ” ( 2 Tim . 3 : 1 - 5 ) Kukhala olimba kuuzimu ndiye kungatithandize kulimbana ndi dzikoli . 14 Tsogolo Lanu Limadalila pa Zosankha Zanu ! ( Yoh . 18 : 33 ) N’kutheka kuti Pilato anali kudela nkhawa kuti mwina Yesu angayambitse msokonezo pa zandale . ( Ŵelengani Masalimo 106 : 43 - 45 . ) Mofanana ndi Baraki , Debora , Yaeli , ndi Aisiraeli odzipeleka 10,000 , kodi nimasonyeza cikhulupililo ndi kulimba mtima mwa kuseŵenzetsa zilizonse zimene nili nazo potumikila Yehova ? ’ Zinali kucitika kuti sin’nali kukopeka naye mtsikana , koma n’nali kuona kuti iye amanikonda . Basi n’nali kuyamba kumaceza naye . ” 2 : 17 ) Ndithudi , dzikoli lidzawonongedwa . Anthu adzasangalala ndi moyo padziko lapansi ndipo sadzakalamba ndi kufa . — Ŵelengani Yohane 5 : 26 - 29 ; 1 Akorinto 15 : 25 , 26 . Kodi dipo idzatheketsa ciani ? DZIKO : ENGLAND Ndam’peleka kwa Yehova masiku onse a moyo wake . ” Ralf amene ali ndi ana anai anati , kulambila kwao kwa pabanja kumakhala ngati kuceza cabe , ndipo aliyense amatengamo mbali . Fotokozani mmene mzimu woyela umatithandizila tikakumana na mavuto . Iye anapempha cilolezo kwa a bishopu kuti andibweze kunyumba ya masisitele ya ku Zaragoza . ( Genesis 1 : 3 ) Mwacionekele , mphamvu ya dzuŵa inadutsa m’mitambo , ndiyeno kwa nthawi yoyamba kuwala kunayamba kuonekela padziko lapansi . 4 : 8 - 10 ) Tikacita zimenezi , tidzaonetsa kuti timakonda Yesu kuposa zinthu zakuthupi . Nanga zioneka kuti iye anathandiza bwanji Paulo ? Adamu atapandukila Mlengi wake , sanakhalenso mwana wa Mulungu . 1 : 7 , 8 ) Ndithudi , limenelo lidzakhala tsiku lapadela kwambili . Fanizo la nkhosa ndi mbuzi linafotokozedwa mu Nsanja ya Olonda ya October 15 , 1995 , tsamba 23 mpaka 28 ndiponso mu nkhani yotsatila m’magazini ino . Seŵelo la Eureka , 8 / 15 Nanga n’ciani cina cacititsa anthu kukhulupilila kuti Mboni za Yehova zili ndi coonadi ? — Ŵelengani Aroma 14 : 17 , 18 . Koma tingacite zimenezi kokha ngati timacita zinthu mogwilizana ndi dzina lathu ndi kukhalabe oyela . Ni zida ziti zimene muona kuti n’zothandiza pophunzitsa ana anu ? Masiku ano , anthu a Yehova akhala akuonetsa cikhulupililo cawo mu Ufumu wa Mulungu . Kupanga zosankha kuli monga kusankha njila yoyenelela mukafika pa mphambano . Timaona Yehova ndi maso a mtima wathu pamene tiphunzila za iye ndi makhalidwe ake Koma anaufotokoza mwa njila imene inam’thandiza kuzindikila chimo lake ndi kucitapo kanthu . — 2 Sam . Koma mosiyana ndi Adamu , Yesu anakhala moyo mogwilizana ndi zimene Yehova anali kuyembekezela kwa munthu wangwilo . Zimene mumakhulupilila : Kodi ni mfundo ziti za makhalidwe abwino zimene nimayendela ? Ngati mumalanga ana anu mwacikondi , moyenela ndi mosasinthasintha monga mmene Yehova amacitila , mungakhale ndi cidalilo cakuti ana anu adzapindula . Ambili anavutika ndipo ena anaphedwa cifukwa ca kukhulupilika kwao . ( Mac . 4 Kukhutila Komanso Kupatsa Ndipo timasangalala tikaona ambili akudzipeleka kuti akatumikile kumalo osoŵa kapena kucitako utumiki winawake , si conco ? M’caka cimene ciletso ca ku Russia cinatha , Matthew wa ku Great Britain anali ndi zaka 28 . Iwo ndi opanda ungwilo ‘ okhala ndi zofooka ngati ifeyo . ’ ( Mac . Mmodzi mwa iwo anali Emil Yantzen , amene anabadwila ku Kyrgyzstan mu 1919 . Zinali zoonekelatu kuti Mdyelekezi anali wokwiya ngako cifukwa ca kaimidwe kamene abalewo anatenga pa nkhani ya nkhondo . Iye anali kusangalala kwambili ndi ulaliki wotelowo cakuti anapanga zolinga zakuti aonjezele utumiki wake mwa kusamukila ku Russia . Kwa zaka zoculuka , wamalondayu ayenela kuti anagula na kugulitsa ngale zambili - mbili . Ndiyeno a Mboni za Yehova anabwela ndipo anafotokoza momveka bwino maulosi ena a m’Baibulo . 28 : 10 - 15 ) Mwa zokamba na zocita zake , Yakobo anaonetsa kuti anali kuganizila kwambili za miyezo ya Mulungu na cifunilo cake . N’citsanzo cabwino citi cimene Timoteyo anaonetsa popititsa patsogolo zinthu za Ufumu ? Njila yacinayi yokuthandizani kulimbana ndi nkhawa , ni kuuzako munthu amene mumam’dalila . Komabe , mwai umenewu sunapelekedwe kwa atumwi 11 okha . ( a ) N’cifukwa ciani Mose anakana “ kuchedwa mwana wa mwana wamkazi wa Farao ” ? 6 : 5 . Komabe n’zotheka kukhalabe wodzicepetsa pa mayeselo . Kukambilana kuli monga biliji , kumakugwilizanitsani ndi ana anu 1 : 22 ) Tikamaganizila zimene Mulungu walonjeza , ndiye kuti tikuganizila zinthu zimene zidzacitika ndithu . — 2 Pet . Ici cinali colinga ca Mulungu . Koma mzimu woyela wa Mulungu unam’patsa mphamvu . Pambuyo pake , Petulo anadzakhala citsanzo cabwino kwa ena . Izi zinatidabwitsa kwambili . Tingaonetse bwanji kulimba mtima pa mavuto ? Cifukwa cakuti apeza mayankho a m’Baibulo okhutilitsa pa mafunso ao . 1 , 2 . ( a ) Kodi Yesu anati lamulo lalikulu laciŵili m’Cilamulo ndi liti ? Ndiye cifukwa cake Yehova analandila nsembe yake . — Ŵelengani Genesis 4 : 3 - 5 ; Aheberi 11 : 4 . N’cifukwa ciani sitiyenela kuda nkhawa tikaona kuti ciŵelengelo ca amene amadya mkate ndi kumwa vinyo pa Cikumbutso cikukwela ? ​ — Aroma 9 : 11 , 16 . Mwina tingaŵelenge lemba limodzi kapena angapo kuti timvetse bwino nkhaniyi . Tiyeni tiyesetse kuti tisagonje pa nkhondo imeneyi , ndipo tidziyang’anitsitsa pa mphoto . Mofanana ndi woyendetsa ndeke ameneyo , Adamu na Hava anasankha kuyenda m’njila yawo - yawo . Amamva bwanji akaona kupanda cilungamo ? 1 / 1 NJILA YOTHETSELA VUTOLI : Mphamvu zoyendetsela Ufumu wa Mulungu ndi zocokela kwa Yehova Mulungu . Okwela pa magaletawo ni angelo ; mwacionekele ndi magulu osiyana - siyana a angelo . ( Genesis 1 : 1 , 2 ) Kodi cinacokela kuti ? Kumbukilani kuti Satana anakaikila kukhulupilika kwa atumiki onse a Yehova . Iye anati sitingakhale okhulupilika kwa Yehova tikakhala pa mayeselo . Mabungwe ambili amaika munthu wina kukhala woyang’anila zocitika zonse . ( b ) Kodi kupanduka kunaonetsa kuti Yehova walephela kulamulila anthu ? Ndiyeno , Petulo anazindikila kuti Mulungu alibe tsankho . Pambuyo pake , adzawonongedwa . ( Chiv . Kodi Akristu anapindula bwanji ndi malamulo a Aroma ? Nanga Ayuda okhala m’maiko ena anathandiza bwanji pa nchitoyo ? Kodi Mumalemekeza Buku Lake la Yehova ? Nthawi zina , Yesu anali kupatsa uphungu atumwi onse cifukwa cokhala ndi ‘ cikhulupililo cocepa . ’ Kuonjezela pa kundithandiza kuti ndikhale ndi umoyo wabwino , Baibulo linatithandizanso kukhala ndi banja labwino . Mwacitsanzo , kodi pali makonzedwe omanga Nyumba ya Ufumu yatsopano imene muzisonkhanamo ? Aliyense wa ife ayenela kudzipenda kuti aone ngati ndi wodzipeleka ndi mtima wonse kwa Mulungu . Nanga bwanji za Yehosafati mwana wa Asa ? ( Ezekieli 33 : 14 - 16 ) Koma popeza kuti Ahabu anaonetsa kukhumudwa pang’ono ndi zimene anacita , Yehova anamucitila cifundo pang’ono . Ayuda anali kuidziŵa mfundo imeneyi na kuivomeleza . Ndiye cifukwa cake iwo anavomeleza kuti Khristu ni mbadwa ya Davide , mwana wa Jese wothela . — Mat . ( Chivumbulutso 6 : 2 ) M’masomphenya , mneneli Danieli anaona Mesiya wooneka monga “ mwana wa munthu ” akupatsidwa “ ulamulilo , ulemelelo , ndi ufumu . ” Tsiku lina , tidzacita Cikumbutso cothela . 34 : 6 , 7 . Masomphenya amenewa ni ulosi umene unakwanilitsika koyamba patapita zaka 5 , panthawi imene Yehova analola asilikali a Babulo kuwononga mzinda wa Yerusalemu . Ganizilani kudela kumene mumakhala , anthu a kumeneko , ndi zimene zimawadetsa nkhawa kwambili . N’ciani cidzacitikila zinthu zoŵelenga ndiponso zoonelela zoipa ? Kodi ifenso sitiyenela kunyadila koposa pokhala ndi mwai wodziŵidwa ndi Yehova , Mphunzitsi Wamkulu ? ” Conco , potengela citsanzo ca abale athu a m’zaka za m’ma 1900 , tiyeni ticite ciliconse cotheka kuti tithandize anthu amenewo kumasuka . Mariya atabeleka Yesu , Yehova sanapatse mtsogoleli aliyense wochuka kapena olamulila a mu Yerusalemu ndi Betelehemu mwayi wodziŵa za kubadwa kwa Yesu . Conco , Danieli sanasinthe cizoloŵezi cake olo kuti izi zinaika moyo wake paciopsezo . Iye sanafune kucita zinthu zoonetsa ngati kuti wayamba kugonja pa kulambila kwake . Iyi ni mbali yofunika kwambili pa nchito yolalikila uthenga wabwino wokamba za kukoma mtima kwa Mulungu . Mungakambilanenso nawo malangizo othandiza ali pa Agalatiya 5 : 19 - 23 . Yonatani analimbikitsa Davide kudalila Yehova . Yehova wakhala akuthandiza anthu ake kupilila kupyolela mu mpingo wacikristu . Hosi yoyela ni cizindikilo coyenelela ca nkhondo yacilungamo yomenyedwa na Mwana wa Mulungu , cifukwa m’Malemba kala yoyela imaimila cilungamo nthawi zambili . — Chivumbulutso 3 : 4 ; 7 : 9 , 13 , 14 . “ Kuwawidwa mtima konse kwa njilu , kupsa mtima , mkwiyo , kulalata ndiponso mau acipongwe , ” zimaika cikwati pangozi . ( Aef . 4 : 31 ) Zoonadi , kulankhula mau osuliza ndi oipa kumaononga cikwati . Kaya tili na zaka zingati , kapena luso labwanji , tonse timalakwitsa . Koma kodi cingakhale canzelu kuthamangila kutsogolo kwa galimoto imene ikuyenda kuti ikugundeni pofuna kudziŵa mmene imaphwetekela kapena kuti muone ngati ingakupheni ? 8 Kodi Pali Amene Akumvetsela ? 9 Timayesetsa kutengako mbali mu ulaliki nthawi zonse Kuthetsa Mkangano ndi Kulimbikitsa Mtendele , June Yosefe amene anali mnyamata wokongola kwambili anazindikila kuti mkazi wa bwana wake anali kumufuna , ndipo zimenezi zinacitikila ku nchito . Cifukwa Baibo na zimene zakhala zikucitika masiku ano , zimatithandiza kudziŵa zimene wokwela pa hosi aliyense akuimila . Petulo atalalikila Koneliyo ndi banja lake , iwo analandila mzimu woyela , olo kuti sanali odulidwa . ( Yer . 10 : 23 ) N’zoona kuti analengedwa na ufulu wodzisankhila zocita , ndipo palibe cikanawaletsa kusankha kudzilamulila okha popanda Mulungu . Komabe , colinga cawo cinasintha pamene anayamba kuŵelenga zofalitsa za Ophunzila Baibo ndi kugwilizana nawo . ( Yak . 5 : 14 , 15 ) Mwacitsanzo , m’bale wina wa ku Italy amene wapilila matenda osacilitsika amene amamufooketsa ndi kumuwondetsa anati : “ Cikondi cimene akulu amandionetsa pondicezela kaŵilikaŵili cimandilimbikitsa kupilila . ” ( Yesaya 61 : 1 , 2 ) Monga mmene malemba anakambila , Yesu anathandiza kwambili anthu amene anali “ kugwila nchito yolemetsa ndi olemedwa . ” — Mateyu 11 : 28 - 30 . Malinga na ciŵelengelo cina , zioneka kuti pakati pa caka ca 1975 na 2000 , zivomezi zinapha anthu 471,000 . Ndipo Malemba amakamba za Akristu odzozedwa kuti ndi “ mkazi ” wa Kristu , “ namwali woyela ” amene walonjezedwa kukwatiwa ndi Kristu . — Chiv . Abale ena anapeleka ndalama zocilikiza nkhondo , ndiponso analipo ena amene ananyamula mfuti na kuyenda ku nkhondo . Kuseŵenzetsa zimene mwaŵelenga M’kupita kwa nthawi , matanthauzo a mau a m’zinenelo zimene zinagwilitsidwa nchito polemba Baibo , akhala akusintha . Yehova atalenga anthu oyamba , iye anawauza kuti : “ Mubelekane , muculuke , mudzaze dziko lapansi , ndipo muliyang’anile . Muyang’anilenso nsomba za m’nyanja ndi zolengedwa zouluka m’mlengalenga , komanso colengedwa ciliconse cokwawa padziko lapansi . ” ( Gen . Kodi n’ciani cinamuthandiza ? Umu ni mmene Mulungu anatilengela . ( Onani palagilafu 13 - 17 ) Kulikonse kumene anthuwo anapita , anali kulambila milungu yao yonama ndi kudzilamulila okha . — Gen . Nthawi zambili , maofesi a nthambi amalandila makalata kucokela kwa abale ndi alongo opempha malangizo a cithandizo ca mankhwala cimene io angatsatile . 19 : 7 . Bungwe Lalikulu la Ayuda limene likuchulidwa apa ni Sanihedirini , kapena kuti khoti lalikulu la Ayuda . Ngati anawathandizadi , ndidziŵa bwanji kuti inenso adzandithandiza ? Nimakondwela kuonana ndi ophunzila ocokela m’maiko osiyana - siyana padziko lonse Coyamba , osafulumila kuganiza kuti udziŵa zimene ena amakhulupilila . Msonkhanowo unatilimbikitsa kwambili ndi kutithandiza kupilila ziyeso zimene zinali kubwela mtsogolo . Zilizonse zimene amatiuza kucita zimatipindulitsa ndi kutipatsa cimwemwe cosaneneka , ngakhale kuti nthawi zina tingafunike kudzimana zinthu zina . — Ŵelengani Yesaya 48 : 17 . Conco , pamene mkulu wanga ananena kuti adzandilipilila maphunzilo a ku yunivesite , ndinaona kuti unali mwai waukulu . Buku lina limati , Aiguputo anamuona kukhala “ wanzelu ndi wamphamvu kuposa zamoyo zonse . ” N’ciani cina cimene cimathandiza kwambili potonthoza ena ? Kodi mudzakhumudwa ngati mkulu mosaganiza bwino wakamba mau amene akukhumudwitsani ? Kodi n’ciani cingakuthandizeni kupilila ? Anthu 1,000 anapezeka pa Msonkhano Wadela umene unacitika ku Mexico City , mu 1941 . Popeza ndife ana a Adamu , timafa cifukwa iye anacimwa . Trazel Popeza anali dokotala , m’mabuku amene analemba , muli nkhani zambili zokhudza kucilitsa kumene Yesu anacita . Iwo analengeza kuti Baibo ya Latin Vulgate ndiyo Baibo yokha yololeka , ndipo anacita zimenezi kwa zaka zambili . Marita ndi m’bale wake . ” ( Yohane 11 : 5 ) Mau amenewa aonetsa kuti Marita anamvela uphungu umene Yesu anamupatsa mwacikondi , ndipo anatumikila Yehova mokhulupilika kwa moyo wake wonse . Mwamsanga iye anameta bwinobwino tsitsi ndi kusintha zovala . Iye ayenela kuti anacotsa tsitsi lonse cifukwa cakuti ndiye cinali cikhalidwe ca Aiguputo . TSAMBA 16 • NYIMBO : 51 , 91 ( Yobu 14 : 13 , 15 ) Yobu anali ndi cidalilo cakuti Mulungu adzamukumbukila ndi kumuukitsa . Iye anadziŵa kuti Davide anali ndi mtima wabwino . Italy 250,000 Kukamba zoona , nthawi zina n’nali kukhumudwa ndipo n’nafuna kuleka kusonkhana cifukwa sin’nali kumvetsetsa zimene zinali kukambiwa , ndiponso n’nali kuona ngati anthu ogontha sanali kuganizilidwa . Pambuyo pake , tifunika kutengelapo phunzilo pa zolakwa zathu , kupitiliza kutumikila Yehova , ndi kuyang’ana kutsogolo mwacidalilo . — Aheb . 2 : 15 - 17 ) N’ciani cingatithandize kupitilizabe kuyenda ulendowu ? Akuwathandiza kulalikila coonadi padziko lonse , ndipo ni iwo okha amene akugwila nchito imeneyi . ( Mateyu 7 : 15 ) Inde , anthu ambili asoceletsedwa . — Ŵelengani 1 Yohane 5 : 19 . Bungwe la akulu lililonse liyenela kuonetsetsa kuti pampingo pali ndandanda ya kuyeletsa pa Nyumba ya Ufumu ndi zipangizo zokwanila zogwilitsila nchito . 5 : 2 . Tikamapemphela kwa Yehova nthawi zonse , timakhala ndi mtendele woculuka wa mumtima ndipo ubwenzi wathu ndi iye umalimba kwambili . Cifukwa cimodzi n’cakuti Mulungu ndi wapamwamba kwambili kuposa anthu . Pamisonkhano , Kingsley anali kukhala pafupi kwambili ndi zokuzila mau ndi kumvetsela mosamalitsa ndiponso kutengamo mbali mwa kuyankha . Ngati taona kuti wina wacita cabwino , n’kulekelanji kumuyamikila ? N’ciani cina cimene tingacite kuti tizigwilitsila nchito bwino Mau a Mulungu mu ulaliki ? Zikusonyeza kuti Yesu , amene tsopano ndi Mfumu kumwamba , ali ndi mphamvu ndipo ndi wofunitsitsa kuthetsa matenda . Iye anati : “ Zili conco ngakhale kuti Baibulo inalembedwa ndi anthu 40 . M’maiko ena , nchito yolalikila kunyumba ndi nyumba imagwilika bwino m’masana kapena m’mazulo . Koma anthu ena amaona kuti n’zosatheka kuti Mulungu angafune kuti awayandikile . Iwo amaona kuti ndi osayenelela kumuyandikila kapena kuti iye ali kutali kwambili . Ninapita , ndipo ninasangalala kwambili . Anthu mu Isiraeli anali ogaŵikana cifukwa ca cidani na tsankho . ANTHU ena anamvapo mwambi wakuti : ‘ Munthu amaona kufunika kwa citsime madzi akauma . ’ Anakhuthula makobidi a osintha ndalama na kugubuduza matebulo awo . ’ M’bale Harry Peterson anali wacangu kwambili pa ulaliki ( Chiv . 4 : 11 ) Kudzicepetsa kumatithandiza kukhutila ndi nchito imene Mulungu anatipatsa , ndi kuiyendetsa bwino . Kodi tiyenela kuwaona bwanji ? Nanga n’ciani cimene Farao anafunika kucita ? 11 : 28 ) Koma kodi tingacite ciani ngati nkhawa zatikulila msinkhu ? 11 : 2 - 21 ) Kwa zaka zambili , Davide anali wokhulupilika kwa Yehova ndipo anali kucita zinthu mwacilungamo . N’kutheka kuti kwa zaka zambili mwakhala mukuyesetsa kuti musinthe , koma mwalephela . Makolo anga anacita cidwi ndi mmene a Papparizos anali kufotokozela Malemba , ndipo anayamba kupezeka pamisonkhano ya Ophunzila Baibo m’mudzi wathu . ( 1 Akor . 5 : 11 - 13 ) Kucotsa wolakwa mumpingo kumacititsa kuti dzina la Yehova lilemekezedwe , kumateteza mpingo woyela wacikristu ndipo kungamuthandize kuzindikila chimo lake . — 4 / 15 , masamba 29 - 30 ( Yohane 11 : 5 ; 19 : 25 - 27 ) Nanga n’cifukwa ciani Yesu anali kum’konda Marita ? Kuyambila kale , Tony ndi Wendy anali okonzeka kupeleka nyumbayi kwa apainiya aliwonse amene ali mu utumiki wa nthawi zonse . 6 : 33 ) Conco , nthawi zonse Akristu oona amasankha kucita cifunilo cake . Koma zolakwa zimenezo sizinasinthe coonadi ca m’Baibo . Ngati n’conco , n’cifukwa ciani ? Mabomba amene ndeke zinali kuphulitsa anali kuchedwa doodlebugs . Anakonzanso zakuti nthawi zina azicitako upainiya wothandiza . N’ciani cingacititse kuti tikhale ndi maganizo ofooketsa ? Mwacitsanzo , mzimayi wina wacikulile anafunsa mphunzitsi wake wa Baibo ngati kunalidi kofunika kuti abatizikenso . Mothandizidwa ndi Yehova , Yosefe anazindikila mwamsanga tanthauzo la lotolo . Iye analota ngala za tirigu 7 zazikulu bwino zikutuluka paphesi limodzi . Kenako anaona ngala zina 7 zikutuluka pambuyo pa zoyambazo . Yehova amafuna kuti aliyense wa ife akhale wololela ndiponso woganiza bwino 5 : 12 ) Alongo ena anacilikiza abale okhulupilika amenewa . Lomba funso n’lakuti , n’ndani amene ali woyenela kutiikila malamulo acilungamo , oyenelela , komanso osapondeleza ? Kodi banja lina linagwilitsila nchito bwanji lemba la Aroma 14 : 2 - 4 ? Kodi munaphunzila mfundo yocititsa cidwi pa phunzilo lanu laumwini kapena la banja ? Kuti banja lizisangalala ndi kulambila kwa pabanja , makolo acikristu aona kuti ndi bwino kucititsa aliyense kukhala womasuka . 24 : 15 ) Kunena zoona , anthu odzipeleka kwa Yehova ali ndi ciyembekezo cosangalatsa kwambili . ( b ) Ni zolinga monga ziti zimene wacicepele angakhale nazo akali wamng’ono ? 25 : 37 - 42 . Aliyense amene amacita “ ntchito za thupi ” ni munthu wakuthupi . ( Agal . Kuganizila mfundo imeneyi kumandicitisa nthumanzi kwambili . ” Baibulo linayamba kulembedwa ku Middle East zaka 3,500 zapitazo . Yesaya analemba ulosi umene unakwanilitsika m’nthawi yake , koma kukwanilitsika kwake kwakukulu kukucitika masiku ano . Ulosiwo unati : “ Anthu amene ali ndi mtima wosagwedezeka mudzawateteza powapatsa mtendele wosatha , cifukwa amadalila inu [ Yehova ] . ” — Yes . 26 : 3 ; ŵelengani Aroma 5 : 1 . Mosakaikila , timasangalala kuti Mulungu walonjeza moyo wosafa wakumwamba kwa odzozedwa okhulupilika ndiponso moyo wosatha padziko lapansi kwa “ nkhosa zina ” za Yesu zokhulupilika . ( Yoh . 10 : 16 ; 17 : 3 ; 1 Akor . Conco , n’nali kupita nawo kukalalikila . Koma ndine wokonzekanso kusintha malinga na zimene Yehova anganipemphe kucita . Anamuuza kuti : “ Ukhale wolimba mtima ndipo ucite zinthu mwamphamvu . Kuli bwanji ise anthu opanda ungwilo ! Anthu ambili m’dzikoli amakonda kukhala ndi zinthu zambili za kuthupi , kulandila malipilo oculuka , kukhala ndi nyumba yabwino kapena zipangizo zina za makono . Conco , anapempha mtumwi Filipo kuti ngati n’kotheka , aonane ndi Yesu . Cikondi cimeneci cikutanthauza kuti ife sitinakonde Mulungu , koma iye ndi amene anatikonda . ” — 1 Yohane 4 : 9 , 10 . Mosapita m’mbali , Mose anagwilitsila nchito maphunzilo a kuuzimu kupititsa patsogolo cifunilo ca Yehova . Kumapeto a mlungu , tinali kukonda kupita kukagonela kuthengo m’matenti , titavala mayunifomu , ndiponso tinali kucita pelete motsatila kulila kwa ng’oma . Apa mfundo ni yakuti , ngakhale kuti inu na m’bale muli na zibadwa zosiyana , n’zotheka ndithu kukhala ogwilizana ngati muyang’ana zabwino mwa iye . Ndimapempha Mulungu kuti andikhululukile ndi kundithandiza kukhala Mkristu wabwino . ” — Magdalene , wa ku Ghana . Iye anapempha Yehova kuti am’kumbukile popeza anayenda mokhulupilika pamaso pake . M’masomphenya amenewa ofotokoza za ulemelelo wa Yehova , Mulungu Wam’mwambamwamba , amene mtumwi Yohane ndi Mneneli Ezekieli anaona , munali zinthu zimene tingakwanitse kuona . Zinthu monga miyala yonyezimila modabwitsa , utawaleza , ndi mpando wacifumu wokwezeka . Kumbukilani kuti nayenso ni bwenzi la Yehova . Ndi mafunso ati amene tifunika kuwaganizila mozama pokambilana pemphelo lacitsanzo ? Ndinawafunsa kuti , “ N’ciani cija ? ” Panthawiyo , zinaoneka ngati kuti mzindawo sudzamangiwanso . — Ezara 4 : 21 - 24 . 8 : 23 . Pambuyo pophunzila naye mitu itatu m’buku la Baibo Imaphunzitsa , Katherine anayamba kudela nkhawa . 25 : 1 - 13 ) Kodi Yesu anafuna kuti ophunzila ake m’masiku otsiliza azilimva bwanji fanizo logwila mtima limeneli ? Kucokela pamene nkhani ya mu 1979 inafalitsidwa , kodi sayansi ya zacipatala yapita patsogolo motani pa nkhani yoseŵenzetsa tuzipangizo twa IUD ? Kenako , mu ulosi umodzimodziwo , Yesu akufotokozanso fanizo la anamwali 10 . Kodi adzapitiliza kum’konda ? Tikagwila nchito , nthawi zambili anali kutilipila madola atatu pa tsiku . Tinatumikila m’dela kwa zaka 12 , ndipo pambuyo pake tinatumikila m’cigawo kwa zaka 21 . N’zolimbikitsa kuona kuti io amakuona kukhala kofunika kwambili . Zimenezi zandithandiza kuti ndiziona Kulambila kwa Pabanja kukhala kofunika . Koma cifukwa ca ukalamba , sakwanitsa kucita zimene anali kucita kale . Iye analemba kuti : “ Pakuti ndinalamulidwa kutelo . Muziseŵenzetsa zida zothandiza pophunzila zimene tili nazo kuti mupeze mfundo zothandiza . Natumikila m’dziko lacilendoli kwa zaka zoposa 60 . ▪ “ Tionjezeleni Cikhulupililo ” N’zotheka kuyamba kum’khulupilila kwambili . N’ciani cimaonetsa kuti Yesu amakonda kwambili anthu ? Anthu amene anali kukhala nao kumeneko anali kulambila akufa , kupembedza mafano , ndi kucita zinthu zina zambili zimene Mulungu amadana nazo . Yehova anandithandiza kuongolela maganizo anga ndi kudziŵa zoyenela kucita ( Yobu 12 : 7 - 9 , 13 ) Pa nthawi ina , onse aŵili , Elihu na Yehova , anaseŵenzetsa zacilengedwe pokumbutsa Yobu kuti Mulungu ni wamkulu kwambili poyelekezela na ise anthu . Ndipo mau otsilizila a ulosi umenewu ayenela kukhudza Mkhiristu aliyense payekha . Atate wathu wakumwamba akutiuza kuti : “ Ineyo Yehova ndidzafulumizitsa zimenezi panthawi yake . ” ( 2 Akorinto 10 : 15 ; Yohane 8 : 29 ) Cikhulupililo cotelo , n’cimene cimathandiza Janet kulimbana ndi nkhawa . Tiyelekezele kuti anthu amene asankha kudzilamulila alinso na moyo wosatha . Iye anali na cikhulupililo mwa Mulungu cifukwa ca zimene anaphunzila ndi zimene zinam’citikila paumoyo . 31 : 1 , 6 , 31 . Zimenezi zikanacititsa kuti azingokhala n’kumadandaula . N’zokondweletsa cotani nanga , ‘ kulemekeza Yehova ndi zinthu zathu zamtengo wapatali . ’ N’coyamikilikanso kuona kuti zopelekazo amaziseŵenzetsa bwino pa nchito yaikulu imene siinacitikepo n’kale lonse . — Miy . Imeneyi ndiyo mfundo yaikulu ya lemba la Salimo 45 . 2 : 8 . * — Deuteronomo 18 : 10 - 12 . ( Sal . 36 : 9 ) Ifeyo monga ana ake aumunthu , timafanana ndi Mulungu m’njila zambili . Sebina anali kapitawo “ woyang’anila nyumba ya mfumu . ” Mwina mfumuyo inali Hezekiya . M’fanizolo , Yesu analimbikitsa ophunzila ake ‘ kupitiliza kubala zipatso zambili , ’ kutanthauza kupilila polalikila uthenga wabwino wa Ufumu . — Yoh . 15 : 8 . Yehova Amatisamalila ndi Kutiteteza Iwo anati : “ Timaona utumiki wathu watsopano kukhala wokondweletsa koma umafuna kulimbikila . Mwacitsanzo , pokhala Akristu timayesetsa kutsatila malangizo a m’Baibulo akuti ‘ nthawi zonse mau athu azikhala acisomo . ’ 35 : 15 , 28 . ( Yohane 21 : 7 ) Nanga n’cifukwa ciani sanacite zimenezo ? Mwina anthu ena sangadziŵe maganizo athu na zocita zathu , koma Yehova amaona zonse ndipo amadziŵa ngati timam’tumikiladi mokhulupilika kapena ayi . — Ŵelengani Yeremiya 17 : 9 , 10 . Iye anafelanso onse kuti amene ali moyo asakhale moyo wongodzisangalatsa okha , koma akhale moyo wosangalatsa amene anawafela n’kuukitsidwa . ” — 2 Akor . Zinthu m’dzikoli zikuipila - ipila , ndipo nchito yolalikila ikupita patsogolo . Conco , kuphunzitsa ena n’kofunika ndipo kuyenela kucitidwa mwamsanga . Khalidwe lathu : Petulo anazindikila kuti khalidwe labwino n’lofunika kwambili . Zocitika za mu umoyo wanga zimanisonkhezela kupitiliza kulengeza za Yehova , amene kwa iye “ zinthu zonse n’zotheka . ” — Mat . Kodi anthu ambili anakhudzika motani ndi khalidwe la Mboni za Yehova panthawi ya nkhondo ? M’masophenya a Ezekieli , kodi mwamuna amene anali ndi kacola ka mlembi , konyamulilamo inki na zolembela , ndiponso amuna 6 onyamula zida zophwanyila , amaimila ndani ? Kuonjezela apo , amadziŵa kuti ife ndi banja lathu tifunika malo okhalapo . Yang’anani anthu , yang’anani nkhope zawo . ( Luka 3 : 38 ) Ndipo Yesu anatiphunzitsa kuti tiziitana Yehova kuti “ Atate wathu wakumwamba . ” Pali Mabaibulo ambili amene amasulidwa , ndipo ena ndi olondola kwambili kuposa ena . Patapita nthawi , Aisiraeli anagwilila nchito limodzi pomanga cihema , ndipo posamuka anali kucipasula ndi kukacimanga pa malo ena . Kuti Yehova akutetezeni , muyenela kudziŵa zimene zimam’kondweletsa ndi kuzicita . Mose sanafunikile kuopa cifukwa anatumidwa ndi Yehova . Conco , makolo sayenela kuganiza kuti ana ao acinyamata ndi osaganiza bwino , kapena amacita zinthu mwacibwana . Mfundo ya m’Baibulo imeneyi yathandiza anthu ambili kuyambanso kukhulupilila Mulungu . Kenako panacitika zinthu zosayembekezeka . Mvula ikagwa pambuyo pa cilala coopsa , mizu ya citsa couma ca mtengo wa maolivi imaphuka n’kumela “ nthambi ngati mtengo watsopano . ” — Yobu 14 : 7 - 9 . Mosakayikila , mukumbukila anthu ena ochulidwa m’Baibo amene anadziletsa atakumana ndi ziyeso . ( a ) Kodi zinenelo zimasintha bwanji m’kupita kwa nthawi ? Christian ndi Daniela ali ndi ana aŵili acitsikana . Pamisonkhano , Mulungu amatithandiza ndi mzimu woyela . 30 : 19 , 20 ) Kuti tikhalebe ndi moyo , tiyenela kucita cifunilo ca Yehova , kum’konda , kumvela mau ake ndi kumamatila kwa iye . 8 : 30 , 31 ) Nanga zikanatheka bwanji kupulumutsa anthu ? Mike anacepetsanso nambala ya makasitomala ake , ndipo anapeza njila imene angaziyendetsela bizinesiyo ali ku dziko lina kupyolela pa intaneti . Mofanana ndi Paulo , ningakambe motsimikiza kuti : ‘ Pa zinthu zonse , ndimapeza mphamvu kucokela kwa iye amene amandipatsa mphamvu . ’ ” — Afilipi 4 : 13 . Yesu anaika “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” kuti azipeleka “ cakudya [ cakuuzimu ] pa nthawi yoyenela ” kwa otsatila ake . ( 2 Mbiri 36 : 13 ) M’malomwake , iye anakapempha thandizo ku Iguputo poyesa kudziombola mu ukapolo wa Babulo , koma sizinaphule kanthu . — Ezek . M’madela ena , kucita zimenezi ndi mlandu wofanana ndi kufalitsa zithunzi za malisece za ana . Kumeneko , Danieli anali kukhala ndi anthu amene sanali kumvela malamulo a Mulungu . Mose anaona dzanja la Yehova pa nkhaniyo . Iwo anapita patsogolo mwamsanga ndipo anabatizika mu 1957 . 10 : 16 ) Patsikulo , abale anali kubwela kusanga m’tumagulu tung’onotung’ono kuti asonkhane . Bwanji osapatula kanthawi koŵelenga na kusinkha - sinkha mau a m’pemphelo limenelo , na kuganizila zimene likutiuza ponena za Danieli ? Mosasamala kanthu ndi zimene Mulungu anawacitila , Mose anadziŵa kuti io adzacita zoipa . 10 : 38 ) Kuti akhale oyenela Khristu , ophunzila ake akhala akupilila mavuto monga kunyozewa , kapena kusankhiwa na anthu a m’banja lawo . Pomvela malangizo a anzakewo , iye anasankha kucitila nkhanza anthuwo . Kwa abale amene anasamukila ku maiko ena , zinawavuta kuzoloŵela nyumba zatsopano , kuseŵenza ndi abale ndi alongo acilendo , ndipo mwina kuphunzila nchito zatsopano . ( Aroma 6 : 9 , 11 ) Umoyo wawo sunali monga mmene unalili kale . Kucita zimenezi kunam’thandiza kuyamikila mwayi wochedwa na dzina la Mulungu . Kodi kukonda coonadi kwatithandiza kuzindikila mwayi wapadela umene tili nawo wodziŵika na dzina la Mulungu ndi kulengeza za Ufumu wake m’nthawi ya mapeto ino ? N’ciani cingatithandize kukambitsilana Malemba mwaluso ? Sitikukaikila kuti Yesu anakhalapo ndi moyo kenako n’kufa . Nanga pali umboni wotani wotsimikizila kuti anaukitsidwa ? Patapita zaka 7 , m’bale Atsushi , mmodzi wa apainiya apadela amene ndinali kutumikila nao pampingo , ananditumila kalata . Kodi pali wacikulile wina amene afunikila thandizo la mayendedwe popita ku misonkhano , muulaliki , ndi ku cipatala ? Iye atatumikila monga mneneli kwa zaka 50 , “ anadwala matenda amene pamapeto pake anafa nawo . ” Kukambilana kotelo kudzatithandiza kum’dziŵa bwino Yehova , ndipo cikondi cathu pa iye cidzapitiliza kukula . — Yohane 17 : 3 . NTHAWI zambili , timakonda kutengela zocita za anthu amene timakonda . Koma mungadziŵe bwanji zosoŵa za munthu ? Kodi mwacibadwa , ise tonse timafuna ciani ? Nkhani imeneyi inanilimbikitsa kuti nidzipeleke kwa Yehova . Sitinali kucitila zinthu limodzi monga banja . Yosiya anayesetsa kucita zinthu zokondweletsa Mulungu kuposa mafumu ambili a Yuda . Abale masauzande ambili apewa ciyeso cimeneci , conco nafenso tingakwanitse . — 1 Akor . “ Anthu Amene Mulungu Wao Ndi Yehova ” Mu mpingo wa ku Korinto munalinso vuto lina . ( Aroma 13 : 3 , 4 ) Mulungu amatiuza kuti tizipemphelela olamulila n’colinga cakuti tikhale ndi mwai wom’lambila mwamtendele . Komabe , pambuyo pa Pentekosite wa mu 33 C.E . , olambila oona sanafunikenso kutsatila Cilamulo ca Mose . ( Mac . 15 : 28 , 29 ; Agal . Pambuyo pake , tinalalikila m’mudzi wonsewo , ndipo tinakondwela kuona kuti anthu a kumeneko anali acidwi ngako . Komabe , kuyambila kale anthu onse a Mulungu , kaya ndi odzozedwa kapena a “ nkhosa zina , ” akhala akupindula ndi “ zinthu zonse zimene zinalembedwa kalekale . ” — Yoh . 10 : 16 ; 2 Tim . Nanga Gogi wa Magogi ndani ? Iye anakamba kuti “ amuna 10 ocokela m’zilankhulo zonse za anthu a mitundu ina , ” amene mophiphilitsa adzagwila covala ca Mwiisiraeli wa kuuzimu , ndi kukamba kuti : “ Anthu inu tipita nanu limodzi , cifukwa tamva kuti Mulungu ali ndi inu . ” — Zek . ▪ Cifukwa Cake Timacita Mgonelo wa Ambuye Imeneyo ndiyo inali nthawi yanga yoyamba kukamba nkhani pa pulatifomu , koma sindinasiye kukamba nkhani m’sukulu . ” Janet Ganizilani lonjezo ili losapita m’mbali lakuti : “ Oongoka mtima ndi amene adzakhale m’dziko lapansi , ndipo opanda colakwa ndi amene adzatsalemo . Araceli : Ndili ku Zaragoza , ndinacita malumbilo oyamba kuti ndikhale sisitele . Pomasulila mau amenewa , omasulila ena amati , mtendele wa Mulungu “ umaposa zonse zimene tingayembekezele , ” kapena kuti “ umaposa nzelu zonse zimene munthu angakhale nazo . ” Kaya mumakhala m’dziko liti , muli ndi mwai wokhala nzika ya Ufumu wa Mulungu . Pofuna kutengako mbali panchito ya Ufumu , Wilhelm Hildebrandt anaitanitsa tumapepala twauthenga twa masamba anayi tochedwa The Bible Students Monthly m’Cifulenchi . Kuphunzila kuona mmene Yehova amaonela zinthu kudzatithandiza kukhala ndi kaonedwe kabwino . ( Luka 4 : 43 ) Yesu anapanga zosankha zimene zinam’thandiza kuika maganizo ake panchitoyo ndi kukwanilitsa utumiki wake . Zimenezi zinatipangitsa kutsimikiza mtima kuti tisamukile m’dzikoli . ” Lameki anakamba zokhudza mwana wake Nowa kuti : “ Uyu ndi amene adzatibweletsele mpumulo ku nchito yathu yopweteketsa manja , cifukwa colima nthaka imene Yehova anaitembelela . ” Iye waona kuti mmene tumapepala tumenetu anatulembela , tumacititsa anthu kukhala ofunitsitsa kukambitsilana . Olo kuti n’nali kuyenda ku chechi na amayi anga mobweleza - bweleza pa Sondo , n’nali kudziŵa zocepa cabe zokhudza Baibo . Ngakhale n’conco , sitifunika kukhala na nkhawa kwambili . “ Kubala zipatso ” kungatanthauzenso kukhala na “ makhalidwe amene mzimu woyela ” umabala . Koma m’nkhani ino na yokonkhapo , tidzakambilana kwambili za kubala “ cipatso ca milomo yathu ” kapena kuti kulengeza uthenga wabwino wa Ufumu . — Agal . N’nakwanitsa kuleka ngakhale kuti n’nali n’tapepa kwa zaka zoposa 10 . Phindu lalikulu kwambili limene timapeza ngati tipeleka ulemu woyenelela kwa ena n’lakuti timakondweletsa mtima wa Mulungu . Koma Wolamulila wathu , Yesu , amatikonda kwambili ndipo amatengela makhalidwe abwino a Mulungu , makamaka cikondi cake . Koma “ dzina lililonse limene munthuyo anachula camoyo ciliconse , limenelo linakhaladi dzina lake . ” — Gen . 15 - 17 . ( Mat . 5 : 8 ) Kuti tikhale ndi maso a kuuzimu amene angatithandize kuona “ Wosaonekayo , ” tiyeni tikambilane citsanzo ca Mose . Iwo anali kuseŵela , kulankhula ndi kuphunzila ndi ana ao . Ana anali osangalala kwambili kuposa mmene analili nkhondo isanayambe . 3 : 5 , 6 ) Ngati tingadziŵe mavuto amene amakumana nawo monga kusankhidwa kapena kusadziŵa bwino cinenelo , tidzaona njila zimene tingawaonetsele cikondi na kuwakomela mtima . — 1 Pet . 9 : 24 . ( a ) Kodi kukhala opatsa kumaonetsa bwanji kuti ndise ‘ anzelu ’ ? Pa cocitika coyamba , iye anacita zinthu moyenela . Kodi iwo akanalandila bwanji thandizo limenelo ? Timalalikila cifukwa cokonda Yehova ndi anansi athu . Conco , yesetsani kupewa kukhala na nkhawa kwambili , mkwiyo wosalamulilika , kaduka , na maganizo ena oononga . Anaika maganizo ake pa utumiki . Iye anati : “ Misonkhano isanayambe komanso ikasila , tinali kucezako na abale na alongo pa Nyumba ya Ufumu . 5 : 9 . Kodi tili na cifukwa capadela citi cokhalila okondwela ? Anthu a ku Filipi anali onyadila kukhala nzika za Roma . ( Mac . N’ciani cingatithandize kuthetsa kusamvana ndi okhulupilila anzathu ? 8 : 22 - 53 ) Komanso , mungasinkhesinkhe za pemphelo lacitsanzo limene Yesu anapeleka . ( Mat . 1 Mbiri 29 : 23 . Tinganene kuti : ‘ Izi siziyenela kucitika m’gulu la Mulungu . ’ Ndithudi ! Kukhala pa ubwenzi na Yesu ni mphatso ya mtengo wapatali . Leka kudzidalila kuti ndiwe womvetsa zinthu . Ngati ndife odzicepetsa , mau athu adzaonetsa zimenezo . Anthu oposa 15,000 anafa . Munthu wina wakale amene anali kufunikila cilimbikitso ni mwana wamkazi wa Yefita . Mwacitsanzo , Aiguputo anali kulambila mulungu wa dzuŵa Ra , wa makumbi Nut , wa dziko lapansi Geb , wa mtsinje wa Nailo Hapi , kuphatikizapo nyama zosiyanasiyana . “ M’masiku a mafumu amenewo , Mulungu wakumwamba adzakhazikitsa ufumu umene sudzawonongedwa ku nthawi zonse . . . . Conco palipano , Yehova walola kuti Satana atiyese . ( Yobu 22 : 29 ) Ndipo n’zoona kuti Mulungu ndi wamkulu kwambili kuposa ise anthu . Tsiku lina , mlendo wina anafunsa kamnyamatako kuti , “ Kodi udziŵa kuti koini yagolide ndiye yamphamvu kuŵilikiza kaŵili ndi ya siliva ? ” * ( Onani mau a munsi . ) — 1 Atesalonika 2 : 13 . Kukambilana zimenezi kutithandiza kudziŵa zimene tingacite kuti tikhale okhulupilika kwa Yehova kuposa kwa wina aliyense . Koma kuti lonjezo limeneli likwanilitsidwe , Yesu anafunikila kufa ndi kuukitsidwa . — Gen . 3 Kodi Malangizo a m’Baibo Akali Othandiza Masiku Ano ? Kuti mupeze yankho dzifunseni kuti : ‘ Ni mavuto aakulu ati amene anthu amakumana nawo masiku ano ? Mwa ici , malinga na mfundo za Kaseŵenzetsedwe ka mawebusaiti athu , mungathe kutumizila munthu wina cofalitsa kupitila pa foni kapena pa tabuleti , kapenanso mungamutumizile link ya cofalitsa ca pa jw.org . Mdani wanu Mdyelekezi akuyendayenda uku ndi uku ngati mkango wobangula , wofunitsitsa kuti umeze winawake . ” Kunena zoona , ndani makamaka amene sakondedwa ndi Yehova ? N’cifukwa cake n’kofunika kwambili kuti tidziŵe zimene fanizoli limatanthauza , ndiponso zimene tifunika kucita kuti tikalandile moyo wosatha . Monga mmene zinalili ku Babulo wakale , “ ansembe acifumu ” odzozedwa sanali kutumikila monga mwa makonzedwe ake . Tifunika kucita ciani kuti Yehova alimbitse cikhulupililo cathu ? Mfundo zomveka ndi zodalilika za m’Mau a Mulungu zinandithandiza kukhala ndi mtendele wa m’maganizo . Ngati ana akhala kutali ndi makolo ao okalamba , thandizo limene angapeleke kwa io lingakhale locepa . Kodi ndili ndi cidwi coŵelenga zofalitsa zatsopano ? Patapita zaka zoposa 20 , n’nalekelatu kutsatila mfundo zimene amayi ananiphunzitsa . 4 : 46 - 54 ) Kodi zinthu zocititsa cidwi zimenezi zikusonyeza ciani ? Izi zinali zosiyana kwambili na maphwando ena acikwati amene tinapitako . Kumeneko , oitainidwa anali kuledzela , kucita zinthu zina zoipa , na kukamba mau onyoza . 40 : 31 . Ngati uonetsa kumuganizila na kumvetsela zokamba zake , nayenso adzamvetsela zimene ukamba . — Tito 3 : 2 . A Zimba : Inenso ndinaŵelenga Baibulo lonse . Taonetsa kope yake imene mwacokela nkhaniyo Tiyeni tione zitsanzo za anthu amene anakumana na mavuto amene tawachula kuciyambi kwa nkhani ino . N’cifukwa ciani Yesu anali kum’konda Marita ? Nanga n’ciani cimene iye anacita cimene cionetsa kuti anali wopanda ungwilo ? Anthu a ku Filipi anali kugona mwamtendele usiku , cifukwa anali kudziŵa kuti asilikali akulonda pa zipata za mzindawo . Koma ngakhale kuti panali zovuta zimenezi , Ophunzila Baibo anacitabe zonse zotheka kuti nchito yolalikila ipitilize . * — Ŵelengani Miyambo 21 : 5 . Anthu ena angalabadile tikapitiliza kuwalalikila moleza mtima Iye wakhala aliko kuyambila kalekale . ” Pamene muphunzitsa wophunzila wanu , kodi mumakumbukila kufunika kwa ubatizo na kukambilana naye za nkhaniyi ? 3 : 1 , 2 . ( Onani ndime 17 ndi 18 ) Yehova anacita zonse zotheka kuti kulambila koyela kusadetsedwe ( Onani palagilafu 16 - 18 ) ( Ŵelengani Chivumbulutso 5 : 9 , 10 . ) N’ciani cimene tikuphunzilapo pa fanizo la kanjele ka mpilu ? Kodi cosankhaco cinali ndi zotsatilapo zotani ? Mai wina anavomeleza kuti : “ Nthawi zina zimandivuta kuti ndicititse kulambila kwa pabanja kukhala kosangalatsa , monga mmene ndimafunila . ” Cidani cimeneci cinakula cifukwa ca zinthu zankhanza zimene n’nacitilidwa m’mbuyomo . ” N’cifukwa ciani analemba zosiyana ? — Luka 3 : 23 ; Mateyu 1 : 16 . Mulungu anaika mwamuna woyamba Adamu m’munda wa Edeni umene unali paladaiso wokongola . Munda umenewu unali ndi nyama zosiyanasiyana . Ababulo anatenthanso ndi moto nyumba zonse zokhala ndi mipanda yolimba kwambili za mzindawo ndi zinthu zake zonse zabwino - zabwino , mpaka zonse zinawonongedwa . ” — 2 Mbiri 36 : 17 , 19 . Pamenepo , tinazindikila kuti gulu limene linakonza nkhaniyo n’limenenso linafalitsa mabukuwo . Lemba la Aheberi 11 : 17 - 19 limafotokoza kuti : “ Mwa cikhulupililo , pamene Abulahamu anayesedwa , zinali ngati wapeleka kale Isaki nsembe . Conco munthu ameneyu , amene analandila malonjezo mokondwela , anali wokonzeka kupeleka nsembe mwana wake wobadwa yekha . Muziwakonda ana anu : Muziwauza ana anu kuti mumawakonda kwambili . Kuti tidzalandile mphatso ya moyo wosatha , tiyenela kupilila mpaka mapeto . Patapita nthawi , mneneli Danieli analimbikila kupemphela ngakhale kuti anali atamuopyeza kuti adzaponyedwa m’dzenje la mikango . Ngati zinatheka mwamuna uja kusintha , n’zothekanso kwa Mkhiristu aliyense masiku ano , maka - maka amene sanacite kufika pa saizi ya munthu wa ku Korinto uja . Iye anaona Ahabu pamene anasankha kucita zoipa ndi kusangalala ndi zinthu zimene anapeza cifukwa ca ciwembu ca Yezebeli . Nanga bwanji ngati tapemphedwa kukapezeka ndi kutengako mbali pa cikwati ca wacibale wathu amene si Mboni , cimene cidzacitikila m’chalichi ? Pamene tipitilizabe kukhala okhulupilika kwa Yehova tifunika kupewa kutengamo mbali m’mikangano ya m’dzikoli . Kugwilitsila nchito zofalitsa za Cituvalu pophunzitsa ena ( Luka 21 : 20 , 21 ) Kodi zimene Yesu anakamba zinacitikadi ? Araceli ali ndi zaka 87 , Felisa 91 , ndipo Ramoni 83 . “ MAYI . ” Komanso abale ena safuna kukalamila maudindo mumpingo . ( 1 Tim . Yobu ananena mau ali pamwambawa zaka 3,000 zapitazo , ndipo akali oona mpaka masiku ano . Khalani na makhalidwe abwino . Muziyamikila abale mocokela pansi pa mtima . 2 : 5 ; 11 : 1 ) Ndiponso timaonetsa kuti tikufuna kukhala m’dziko limene anthu onse azidzamvela Yehova . Iye anamanga mizinda ikulu - ikulu monga wa Babele ndi kudziika kukhala mfumu “ m’dziko la Sinara . ” Nili na zaka 17 , n’nayamba utumiki wa pa Beteli ku Brooklyn 1 : 18 . ( Ŵelengani Mateyu 25 : ​ 1 - 13 . ) Timafunikanso kucita zinthu molimba mtima mumpingo . Cokondweletsa n’cakuti anatilonjeza kuti posacedwa adzacotsapo imfa kwamuyaya , na kuukitsa anthu mabiliyoni amene ali m’cikumbukilo cake . Iye anali kugwilitsila nchito mau osavuta kumva . Munthu wolungama Loti , anali kuzunzika ndi zoipa zimene zinali kucitika m’mizindayo . Tikakumana ndi mavuto ambili , tingaiŵale kuti Yehova anatithandizapo nthawi zambili m’mbuyomu . Adani athu angatiukile na kutigonjetsa panthawi imene tikugona mwauzimu . Conco tifunika kukhala maso nthawi zonse . Mogwilitsila nchito mpingo woona wacikristu , Yesu akuthandiza anthu kukhala ndi umoyo wabwino . ( Aheberi 12 : 11 ) Ngakhale ndi conco , kodi tiyenela kucita ciani Yehova akatipatsa cilango ? N’zosatheka kuti tonse tikhale akulu , apainiya , amishonale , kapena atumiki a pa Beteli . Citsanzo ni zimene analemba mu Aroma caputa 16 . Motelo , kuti tipewe mayeselo tifunika kucita zinthu ziŵili izi : Kuyandikila kwa Yehova ndi kupitilizabe kupempha thandizo lake . Mwa ici , sitiyenela kukayikila ngakhale pang’ono kuti Mulungu , amene analenga dzuŵa lamphamvu conco , angatipatse mphamvu zotithandiza kupilila vuto lililonse limene tingakumane nalo . Buku lina linati : “ Anthu ambili padziko lapansi amalankhula bwino Cingelezi . ” Ndiyeno anamva mthenga wa Mulungu akukamba kuti mtengowo udulidwe . Anyamata amenewa anadalitsidwa kwambili cifukwa cotsatila mfundo zakuuzimu zimene anaphunzitsidwa ali ana . — Danieli 1 : 8 , 11 - 15 , 20 . Mosiyana ndi zimenezi , mzimu wodzimana ungatithandize kulandila thandizo ngakhale kuti zimenezi zingaticititse manyazi . ( Miy . Cilamulo ca Mose cinakamba kuti zonyansa za munthu ziyenela kufoceledwa kutali na malo okhala anthu . — Deuteronomo 23 : 13 . Atandiuza kuti iye ndi mwamuna wake ndi a Mboni za Yehova ndinakondwela kwambili . ( Deut . 19 : 3 ) Malinga ni mbili ya Ayuda , Aisiraeli anali kuika zikwangwani zothandiza munthu wothaŵa kudziŵa kumene kuli mizinda yothaŵilako . Mkazi wina amene anali ndi nthenda yotaya magazi , analoŵa m’khamu la anthu ndi kugwila malaya a Yesu , ndiyeno mkaziyo anacila . Mwa khalidwe lathu ndi mtima wathu . 10 : 34 - 36 . 5 : 8 . Iye ndi wocititsa mantha kuposa milungu ina yonse . Zikakhala conco , n’nali kudandaula , kusoŵa tulo , na kukhala na nkhawa . Munthu wodzicepetsa saiŵala kudalila Yehova ndipo amadziŵa malo ake m’makonzedwe a Mulungu . Yehova adziŵa kuti angelo ndi osiyana kwambili ndi anthu , motelo anasankha anthu kuti alembe Baibulo . 29,185 Kwa nthawi yaitali , iye anali kunithandiza ndi kunipatsa malangizo pa zinthu zauzimu . Ndiyeno , posapita nthawi anayamba kundiphunzitsa Baibulo . Klaus Jensen , amene anali kuyang’anila dipatimenti imeneyo , ananipempha kuti niziyenda na dilaiva wa thilaki yonyamula makatoni a zofalitsa . 8 Tengelani Khalidwe la Yehova la Cifundo Kweni - kweni , zimadalila ngati timayamikiladi cisomo ca Mulungu cotikhululukila zocimwa zathu . Kodi izi zitanthauza kuti kupulumutsidwa kwa anthu n’kosafunika kweni - kweni ndi kuti Yehova satinganizila ? Pamene Kaini anaona kuti nsembe yake sinalandilidwe ndi Mulungu , “ anapsa mtima kwambili . ” Anawonjezela kuti , “ Popeza n’nali kale na nkhawa zambili , sin’nafune kuonjezela nkhawa zina cifukwa ca zinthu zimene sizingacitike , ndipo mwina sizikanacitika n’komwe . ” Yehova amadziŵa zinthu zonse zokhudza mabiliyoni a angelo ndiponso anthu amene iye analenga . Ngati mumatelo , kumbukilani malangizo ofunika kwambili akuti tiyenela kukhala ‘ odzicepetsa , ndi kuona ena kukhala otiposa . ’ — Afilipi 2 : 3 . Mwacitsanzo , pamene Katharina anali na zaka 17 , anadziikila colinga cakuti azilalikila anzake a ku nchito . Iye anali kudziŵa kuti abale ake amamuda kothelatu . Cifukwa cakuti Mulungu anali kum’konda , Danieli anaikidwa kukhala nduna yaikulu mu ulamulilo wa Babulo , komanso mu ulamulilo wotsatila wa Mediya ndi Perisiya . Taganizilaninso citsanzo ca Mfumu Uziya . ( Agal . 5 : 22 , 23 ) Yehova amacita zinthu modziletsa nthawi zonse . Nchito yake yaikulu inali kutumikila Mulungu . Kodi mau amene Yesu anakamba onena za cakudya calelo , ayenela kutikumbutsa ciani cimene ndi cofunika kwambili ? Koma mumtima , anali anthu okonda Mulungu . KODI ndinu Mboni ya Yehova yodzipeleka ndi yobatizidwa ? Ana ake aŵili Frank ndi Francis ni amphundu ndipo ni anzanga apamtima . Ngakhale kuti ena angakusonkhezeleni kukhulupilila ciphunzitso ca cisanduliko , inu muli ndi zifukwa zomveka zokhulupilila zimene Baibulo limanena pankhani ya cilengedwe . Ndife oyamikila kuti Yehova watikokela kwa iye ndi kutithandiza kupanga ubale wolimba ndi kupitilizabe kukhala paubale umenewo ndi iye . Mu 1962 , Sukulu ya Utumiki wa Ufumu ya abale ndi alongo amishonali inacitika m’dziko lonse la Brazil . N’cifukwa ciani Yesu anagwilitsila nchito mafanizo aŵiliwa ? Tifunika kuonetsetsa kuti kupita kwathu patsogolo mwauzimu kukuwonekela kwa “ anthu onse . ” ( 1 Tim . 4 : 15 ; Mat . Tikatelo , anthu adzafuna kudziŵa zambili za Mulungu amene timalambila . Koma zimakhala zovuta kudziŵa tanthauzo la zimene munthu akulankhula ngati zimene akunena sitikuzimvetsetsa . ( 1 Akor . Coyamba , anakamba za “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu , ” kagulu kang’ono ka abale odzozedwa amene anali kudzatsogolela anthu a Mulungu . Kodi phunzilo la Baibulo n’ciani ? Ameneyo anali amai ake amene anamwalila pamene anali kubeleka Benjamini mng’ono wake . Pocita zimenezi , muyenela kutsatila malamulo amene mabanki a m’dziko lanu amayendela . Timoteyo anadziŵa Malemba Aciheberi kuyambila ali wakhanda . Panali malamulo oletsa anthu a mitundu yosiyana kucitila zinthu pamodzi , ndiponso anthu anali aciwawa kwambili . Naboti , ana ake , ndi acibale awo , akadzaukitsidwa pa kuuka kwa olungama , adzaona kuti Yehova ndi wacilungamo . N’cifukwa ciani si nthawi zonse pamene tingatifunike kudziŵa cifukwa cake Yehova amacita zinthu mwa njila inayake ? Pa nkhani imeneyi , Akhristu okwatilana ayenela kumvetsa mmene zipangizozi zimaseŵenzela na kuganizila mfundo za m’Baibo . Kuwonjezela apo , anafutukula mtima wawo mwa kucelezako ena kunyumba kwawo . Kodi Kugwila Nchito Mwamphamvu N’kofunikadi ? Koma Yehova anam’thandiza kukhala na cidalilo . ( Yer . Nili na Eunice mu 1960 ndi mu 1989 ( Eks . 17 : 4 ) Poona zimenezi , Yehova anapatsa Mose malangizo omveka bwino . Kapena ngati tilalikila munthu wosapembedza , tingamufunse kuti , “ Kodi munaumvelapo mwambi wakale uwu ? ” 6 : 2 , 5 , 8 . Ena amaphunzitsa ana awo ang’ono - ang’ono mfundo zosavuta poseŵenzetsa nkhani zimenezi . Kodi nimawalezela mtima abale anga na kuwamvetsetsa ? Mfumu Davide anapempha mwai wocita zimenezi pamene analemba kuti : “ Inu Mulungu , mwandiphunzitsa kuyambila pa unyamata wanga . . . . 10 : 23 . Tikhoza kuona kuti Yehova amatiphunzitsa mwa njila yosavuta kumva . Cikhulupililo cake cinali colingana ndi ca mmishonale uja amene anapatsa banja lathu mabuku . Cifukwa cakuti ndimatenga nthawi yaitali mu ulaliki ndiponso kuphunzila zinthu zina kwa alongo ena , ndaonjezela luso langa pa nchito yolalikila . Kodi Mose anacita ciani Aisiraeli atapanduka pa nthawiyi ? Ngakhale kuti Yehova sayembekezela kuti tizicita zinthu mwangwilo , iye amafuna kuti atumiki ake azitsatila miyezo yake yolungama . Kenako ndinawauza kuti , “ Ndinaliŵelenga kale . ” Yehova adzapitiliza kuonetsa kukoma mtima kwake kwakukulu ngakhale pambuyo pa mapeto a dziko loipali . Yesu analimbikitsanso mzimayiyo mwa kumuuza kuti : “ Cikhulupililo cako cakucilitsa . Mboni zambili zikupindula ndi ulaliki umenewu . Tikaganizila nthawiyo , timamva ngati mmene mtumwi Paulo anamvela pamene analemba kuti : “ Abale sitikufuna kuti mukhale osadziŵa za masautso amene tinakumana nao . . . Analinso kudziŵa bwino Malemba cakuti anali kuyankha mafunso ambili amene tinali nawo . ( Luka 8 : 1 ) Ngakhale masiku ano , n’kofunika kuphunzitsa ena kuti akhale alaliki ogwila mtima . Koma Yesu anaika ‘ kapolo wokhulupilika ’ mmodzi yekha kuti ndiye azigaŵila cakudya cauzimu . Ndi mwai wotani umene anthu a Mulungu ali nao ? Nanga tifunika kucita ciani ndi mwai umenewo ? Ndi nkhani iti imene yakusangalatsani ? Mu Isiraeli , ansembe anali kufukiza nsembe kwa Yehova tsiku ndi tsiku . Enanso angakhale opwetekedwa mtima cifukwa cakuti cikwati cawo cinasila posacedwa . ( Aroma 8 : 6 ) Imeneyi ni nkhani yoopsa — imfa ya kuuzimu tsopano , ndi imfa yeni - yeni m’tsogolo . Ena mwa iwo sangacite zambili potumikila Mulungu poyelekezela na mmene anali kucitila kale . Koma angaonetsebe kulimba mtima ndi kugwila nchito mwamphamvu . Koma ndilibe Baibulo . Monga Akhristu , timakhala okhulupilika kwa anthu amene anatilemba nchito , koma timaona kuti cinthu cofunika ngako ndi kukhala wokhulupilika kwa Yehova Mulungu . Wolemba mbili waciroma wina wochedwa Tacitus , amene analemba za olamulila ufumu wa Roma , anatsimikizila kuti Pontiyo Pilato analamula kuti Yesu aphedwe panthawi imene Tiberiyo anali kulamulila . ( Yohane 13 : 13 ) Iye anali kuphunzitsa gulu la anthu komanso munthu aliyense payekha . Ife tinatengela ucimo ndi imfa kwa Adamu . Anthu a Yehova akhala akuona kuti kuimba ni mbali yofunika pa kulambila kwawo . Iye adziŵa kuti tsiku lililonse timayandikila tsiku limenelo . Mau amenewa anaŵeleŵesedwa kwa mkazi wina dzina lake Bebe . Nkhani ino ikubweletsa funso limene aliyense wa ise afunika kuliganizila mozama . Funso lake n’lakuti : Kodi pali ciliconse — kaya udindo , nchito , cuma , cibululu , kapena ufulu wathu — cimene timaona kuti n’cofunika ngako kuposa ubwenzi wathu na Yehova ? ( Nyimbo 1 : 4 - 14 ) M’busayo anafunafuna kumene kunali mtsikanayo mpaka anam’peza . ( Oweruza 11 : 9 ) Iye anayesetsa kukhala wokhulupilika kwa Yehova . Zotsatila zake n’zakuti zimene timaganiza , kukamba , ndi kucita , zidzakhala zokondweletsa Yehova ndipo tidzaphunzila kulimbana ndi zofooka zathu . N’zothekanso kutumiza nokha zopeleka zanu ku ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova m’dziko lanu . 18 : 13 ; 22 : 24 - 27 ; Yer . Tikuyembekezela mwacidwi nthawi pamene tidzakhala angwilo ndi kutumikila Yehova mpaka kalekale . Mau akuti “ Atate wathu ” osati “ Atate wanga , ” amatikumbutsa kuti tili ‘ m’gulu la abale ’ amene amakondanadi . ( 1 Pet . Tiligu ameneyu anali wovuta kucotsa mankhusu ake . Conco , kupela tiliguyo inali nchito yovuta , ndipo inali kufuna kuusinja mu mtondo kapena kuupela pa mphelo . 12 , 13 . ( a ) Kodi tingawathandize bwanji abale othaŵa kwawo ? ( a ) N’cifukwa ciani anthu a Mulungu anafunikila kuwongolelewa pakati pa 1914 ndi 1919 ? Mukacidziŵa , ciciteni . * ( Deuteronomo 32 : 4 ) Conco tingakambe ciani pamenepa ? NI NTHAWI ya msonkhano wofunika kwambili m’Yerusalemu . Kodi Sara , amene anali wokalamba , anali kuyembekezela kuti Yehova adzamupatsa mphamvu yobeleka mwana ? Motelo , tifunika kukhala osamala kwambili ndi zinthu zimene timaŵelenga , kuonelela , ndi kumva , zimene zingatipangitse kukhala ndi “ zilakolako za dziko . ” — Tito 2 : 12 . N’cifukwa ciani tiyenela kuyembekezela moleza mtima kuti Yehova adzatithandiza pa mavuto athu ? Koma kodi mumaganizilapo za mmene lemba la Aroma 5 : 12 limakhudzila kaimidwe kanu pamaso pa Yehova , zocita zanu , ndi tsogolo lanu ? Malinga ndi fanizoli , anamwali asanu anali anzelu ndipo asanu anali opusa . Ndiyeno iye na Sila analalikila mogwila mtima kwa woyang’anila ndendeyo na banja lake . Apempheni kuti azikupemphelelani . Kodi sindiye zimene timatanthauza tikauza mwana kuti , “ Uzimvela makolo ako ” ? Nanga n’ciani cingathandize Mkristu kukhalabe wokhulupilika kwa Yehova ? ( 1 Tim . 2 : 14 ) Izi zitangocitika , Yehova anayamba kuvumbula zinthu zina zokhudza mdani ameneyu , amene anasoceletsa Adamu na Hava . Ndipo analonjeza kuti pamapeto pake , mngelo woipayu adzawonongedwa . Mokhulupilika , Nowa anagwila nchito yonse imene Yehova anam’patsa . Anthu a kuno sazonda Mboni , ndipo ali na cidwi ngako na uthenga wabwino . ” Masiku ano , zinthu padzikoli zikuipilaipila . Tiyenela kutengela citsanzo ca ophunzila a Yesu okhulupilika kuti tizimvetsetsa tanthauzo la mafanizo ake . Poyamba amayi sanali kudziŵa bwino za khalidwe langa . “ Mwanawankhosa ” amene cikwati cake cidzabweletsa cisangalalo kumwamba ndi Yesu Kristu . ( Yoh . Potengela citsanzo cake , iwo amakambilana ndi amuna awo moona mtima ndi mwaulemu . 12 , 13 . ( a ) N’ciani cinacitikila Yesu atangobatizidwa ? Tili m’sitima yochedwa Queen Elizabeth , pa ulendo wopita ku Sukulu ya Giliyadi Yesu anaukitsidwa ndi kukakhala na moyo wauzimu kumwamba . Ni mmenenso anthu ena adzacitila . Nkhani ya Diotirefe ionetsa kuti anthu odzikuza ndi ofunitsitsa udindo angathe kuyambitsa magaŵano mumpingo . Conco , Yohane anauza Gayo kuti : “ Usamatsanzile zinthu zoipa . ” Baibulo limalonjeza kuti : “ Taonani ! Mosalephela ndidzamumvela cisoni . ” mungapewele mavuto ngati n’kotheka . Ndipo n’cifukwa ciani ? Ngati pacitika zina zake ndipo simukudziŵa coyenela kucita , kungakhale kwanzelu kudzifunsa kuti , ‘ Kodi Yesu akanacita ciani pamenepa ? ’ Ana anu angadziŵe bwanji kuti muli ndi nthawi yolankhula nao ndi kuti ndinu ofikilika ? Kodi acicepele ambili apindula motani ndi Kulambila kwa Pabanja ? Kuyambila nthawi yakale , Yehova wakhala ndi atumiki ake okhulupilika amene amam’tumikila mu utumiki wanthawi zonse , ngakhale kuti amakumana ndi mavuto m’dongosolo lino la zinthu . N’cifukwa ciani nthawi zina kukhulupilila Yehova tikakhala ndi mavuto kumakhala kovuta ? Tikuonetsa kuwala kwathu pa mlingo waukulu kwambili kuposa mmene tinali kuyembekezela . Iye amafuna kuti uthenga wabwino ulalikidwe padziko lonse lapansi , ndipo watipatsa mwai wogwila naye nchitoyi . Ndiyeno , mokondwela iye adzabweza ulamulilo wake kwa Yehova ndi kupeleka kwa iye mtundu wa anthu angwilo . Capakati pa November mpaka pakati pa March , kuyenda panyanja kunali kosaloleka . 16 : 7 ) Kukumbukila mfundo yosatsutsika imeneyi kudzatithandiza kukhala odzicepetsa , kuzindikila kuti sitidziŵa zonse , ndi kusintha maganizo athu pankhaniyo . Koma n’zomvetsa cisoni kuti okwatilana ena amalankhulana mopanda ulemu kuposa mmene amakambila ndi munthu amene samudziŵa kapena ndi ziweto monga galu ndi cona . Cifukwa ca macimo amenewa , Davide ndi banja lake anakumana ndi mavuto aakulu . Komabe , Mulungu amakondwela kwambili ngati tilimbikitsa Akhiristu anzathu ndi ena . ( Miy . Makalata a mtumwi Paulo komanso mabuku ena a m’Baibulo naonso analembedwa m’Cigiriki . Matsue Ishii ndi mwamuna wake Jizo , amodzi mwa akopotala oyamba ku Japan , analalikila pafupifupi dziko lonse , kuyambila ndi dela la Sapporo mpaka ku Sendai , Tokyo , Yokohama , Nagoya , Osaka , Kyoto , Okayama , ndi Tokushima . Mau amenewa anakwanilitsidwa zaka zambili pambuyo pa utumiki wa Yesu wapadziko lapansi . — Ŵelengani Yesaya 13 : 19 , 20 ; 2 Petulo 1 : 20 , 21 . MAKOPE 5,800,000 N’nali Kukonda Baseball Kuposa Cina Ciliconse ( S . 24 Yehova Amatsogolela Anthu Ake m’Njila ya ku Moyo Koma iye sanawauze zakuti azikondwelela Khrisimasi . Koma kugonjela kudzatithandiza kukhala okhutila ndiponso osangalala pamene tikucita cifunilo ca Yehova kulikonse kumene tidzakhale panthawiyo m’dziko latsopano . Nkhani zimene zimapelekedwa , maseŵelo , ndi zitsanzo , zimatilimbikitsa kucita zimene tingathe potumikila Yehova . Nafenso tili ndi nchito . Iye amatilangiza kuti : “ Khala wanzelu ndi kukondweletsa mtima wanga . ” Koma phunzilo laumwini lopindulitsa lili monga ulendo wokaona malo atsopano . Limatipatsa mwayi wofufuza na kudziŵa makhalidwe ena abwino a Yehova . Njila ina imene imathandiza kusintha - sintha nkhani ndi kukhala ndi pulogalamu yocita zinazake , monga kupanga Combo ca Nowa coyelekezela kapena kacisi wa Solomo . Maiyo anayamba kuphunzila Baibulo ndi mlongoyo . Mateyu pamodzi ndi ena , anamvetsela pamene Yesu anali kuphunzitsa panthawi ya cakudya m’nyumba ya Mateyu . — Mat . Kodi makolo acikondi acikhristu angafune kuti mwana wawo aziyendela maganizo a dzikoli pa nkhani ya kukhala na umoyo wabwino ? Kodi makolo afunika kuzindikila ciani ? Ndipo nkhani imeneyi , ni yofunika kwambili kwa Mulungu amene timam’lambila . ( Gen . Yesu anati : “ Aliyense woyang’anitsitsa mkazi mpaka kumulakalaka , wacita naye kale cigololo mumtima mwake . ” ( Mat . 5 : 27 , 28 ; 2 Pet . Yehova wapeleka citsanzo cabwino koposa ca kudziletsa . ( Ŵelengani Mateyu 13 : 34 , 35 . ) Conco , monga makolo , pitilizani kukulitsa cikhulupililo canunso . Conco , Gidiyoni ndi asilikali ake anapitiliza kuthamangitsa adani ao ndipo pamapeto pake anawagonjetsa . — Oweruza 7 : 22 ; 8 : 4 , 10 , 28 . Kamvedwe kakale : Mu 1919 , Yesu anafupa akapolo ake odzozedwa padziko lapansi mwa kuwapatsa udindo woonjezeleka . ( b ) N’ciani cinathandiza mlongo wina kuzindikila kuti anafunika kukakhalanso ndi banja lake ? Ndipo pakangotsala milungu yocepa , timagwila nchito mogwilizana poitanila anthu ku Cikumbutso . Boazi anati : “ Tamvela mwana wanga . ” 1 : 1 , 2 ) Inali nkhani yomumvetsa cisoni powalembela za khalidwe loipa laciwelewele limene iwo anali kulekelela mu mpingo . Kodi mudzacita ciani ngati Akristu anzanu akukhumudwitsani kapena ngati muona kuti akucitilani zinthu mopanda cilungamo ? ( 1 Maf . 15 : 16 - 22 ) Komabe , Mulungu atasanthula bwino - bwino mtima wa Asa , anaona kuti iye “ anatumikila Yehova ndi mtima wathunthu masiku ake onse . ” A Inoki : N’zoona . Palibe munthu wangwilo . Conco , ndinapitiliza kupemphela kuti ndipeze mayankho okhutilitsa . Daniel , wa zaka 21 , anati : “ Ana asukulu anzanga na matica anali kuniseka cifukwa cakuti nimakonkha miyezo ya m’Baibo . Uwu unali mwai umene Aisiraeli akanakhala nao pamene anali kutsogoleledwa ndi Cilamulo . Zimenezi zinamucitikila kuti mwa kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu , alaŵe imfa m’malo mwa munthu aliyense . ’ ( Aheb . Yesu anaphunzitsidwa ndi Atate ŵake kumwamba , koma anaphunzila zowonjezeleka pamene anali kucita utumiki wake pano padziko lapansi . Zimenezo zidzacititsa kuti pakhale nkhondo ya Aramagedo imene idzapangitsa kuti dzina loyela la Yehova lilemekezeke . ( Chiv . 14 : 4 ) Ngakhale ndi conco , Aisiraeli analibe cikhulupililo . Iwo anali kuona cabe Nyanja Yofiila kutsogolo kwao , magaleta ankhondo a Farao amene anali kuwalondola mofulumila m’mbuyo mwao ndi mtsogoleli wao wacikulile wa zaka 80 . 35 : 25 , 26 , 30 - 35 . ( Akolose 3 : 14 ) Conco , ngati mabwenzi ali na cikondi cimeneci onse amakhala otetezeka ndi acimwemwe , ngakhale kuti ni opanda ungwilo . ( 2 Mbiri 19 : 7 ; Malaki 3 : 6 ) Mulungu anatuma Yesu “ kudzalalikila za kumasulidwa kwa ogwidwa ukapolo . . . , kudzamasula opondelezedwa kuti akhale mfulu . ” Pamapeto pake , Mike ndi banja lake anasamukila ku dziko lina , ndipo kumeneko anali kusangalala ndi utumiki wao . Anachula kuti mbeu imeneyo idzacokela m’mbadwa za Abulahamu . Ndi funso lotani limene Habakuku anafunsa Yehova ? Inu ndinu thandizo langa ndi wopeleka cipulumutso kwa ine . ” “ Kodi cipembedzo cimatigwilizanitsa kapena cimatigaŵanitsa ? ” Kodi uthenga waciŵili ndi wogwilizananso ndi kupanduka kumeneko ? Kupitilizabe kupempha kumaonetsa kuti timafunitsitsa thandizo la Mulungu paumoyo wathu . ▪ Muzikumbukila Amene Ali mu Utumiki Wanthawi Zonse Tikaika maganizo athu pa zinthu za “ mzimu , ” tidzakhaladi na umoyo wokhutilitsa ndi watanthauzo ngakhale pali pano . Cifukwa ca ukalamba sakwanitsanso kulalikila kunyumba ndi nyumba . Patapita miyezi yocepa , tinayamba kuvinila limodzi ndi David m’nyumba ina yaikulu yocitilamo maseŵela yochedwa Royal Opera House m’dela la Covent Garden , ku London . Tiyeni tikambilane citsanzo ca kholo lina . Conco , mokoma mtima iwo anam’funsa cifukwa cake iye akulila . Paulo anafotokozanso zabwino ponena za amai a Rufu , mwacionekele cifukwa ca zimene amaiwo anam’citila panthawi ina . Nanga n’cifukwa ciani Lefèvre anali wofunitsitsa kuthandiza anthu wamba kudziŵa zimene Baibo imaphunzitsa ? Ndi mmene Abulahamu nayenso anamvelela . Olo kuti nkhaniyo tiidziŵa bwino , Yehova yekha ndiye amaona mmene mtima ulili . ( 1 Sam . Zimathandizanso kusamalila amishonale , apainiya apadela , na oyang’anila madela . ŴELENGANI NKHANI ZINA PA INTANETI | www.jw.org / nya ( Deuteronomo 18 : 9 , 10 ) Malinga ndi Cilamulo ca Mose , nsembe yopseleza inali kupelekedwa kwa Yehova yekha . ( b ) Kodi Yesu anagogomeza bwanji kufunika kokhala opilila ? Ngati n’conco ndiye kuti boma locokela kwinakwake osati lopangidwa ndi anthu ndi limene lingakhale lopanda ziphuphu . 49 : 10 . 2 : 2 ) Mbali yaciŵili , n’cifukwa ciani acinyamata afunika kukhala aulemu pamene akuthandizila abale acikulile , ndi kuphunzila kwa iwo ? Zimene Davide anakwanitsa kucita : Davide analola Yehova kum’cilitsa mwauzimu . Tingapeze mayankho a mafunso amenewa ndi ena aconco m’Baibulo . Mfumu yakwela pa hachi ‘ cifukwanso ca kudzicepetsa . ’ Komabe , pali cocitika cimodzi capadela cimene Akhristu oyambilila anali kucidziŵa bwino — Cikumbutso ca imfa ya Yesu . Zimenezi zinali kukopa anthu kuti adzagule zipatso . Wandiwelamitsa ndi cisoni . ” ( Gen . 2 : 15 - 17 , 19 , 20 ) Ndiponso , Yehova anapanga Adamu ndi Hava m’njila yakuti adzikwanitsa kulaŵa , kukhudza zinthu , kuona , kumva , ndi kununkhiza . MTSIKANA anathamanga kukalandila atate ake . Kodi ndimatengako mbali ndi mtima wonse pa kulambila kwa pabanja ? ’ Cifukwa ca zimenezi , iye anati , “ Ndinaleka kupemphela . ” TSAMBA 25 • NYIMBO : 22 , 68 Ifenso ndife opanda ungwilo , ndipo tikakumana ndi mavuto ngati amenewo , tikhoza kutengela zitsanzo zabwino za m’Baibulo ndi kupewa kutengela zitsanzo zoipa . Masiku ena mkati mwa mlungu , mwina mungaŵelenge ndi kusinkhasinkha mfundo za m’Baibulo malinga ndi ndandanda ya Sukulu ya Ulaliki . Abulahamu anali kudziŵa kuti Yehova adzaononga anthu amene anali kucita zinthu zoipa . Caka cotsatila , Brian na Kimberly anamanga banja , apo Kimberly anali na zaka 25 . Mabuku ena amanena kuti liu laciheberi lomasulidwa kuti “ cilamulo ” ndi logwilizana ndi liu limene limatanthauza “ kutsogolela ” ndi “ kulangiza . ” Mwina okalamba amangofunikila munthu woŵathandiza nchito zina kuti akhale okha . N’zosangalatsa kwambili kudziŵa kuti kuyambila mu 1919 , Yehova wapatsa anthu opanda ungwilo mwai wogwila naye nchito yopanga paladaiso wauzimu , kuulimbitsa , ndi kuukulitsa pano padziko lapansi . Ndipo kodi anthu inu mudzacita ciani pamapeto pake ? ” Popeza kuti Yehova ndiye Bwenzi lathu la pamtima , kodi tili ndi cizolowezi colankhulana naye m’pemphelo ? * Atamulandila , anamupatsa cakudya , koma iye anakana kudya mpaka atafotokoza cimene anabwelela . 1 : 1 ; 21 : 3 - 5 . ( Mateyu 6 : 33 ) Pamene tiganizila zimene Sara anacita , tingadzifunse kuti , ‘ Kodi n’dzasankha kucita ciani pa umoyo wanga ? ’ Lemba la Chivumbulutso 21 : 4 limati : “ imfa sidzakhalaponso . ” Mwacitsanzo , Adamu anali na zaka zoposa 600 pamene Inoki anabadwa . Ena angakhale kuti amagwilizana na mpingo , koma ni ofooka mwauzimu . Ngati makolo akhala ndi mavuto monga amenewa , mwamsanga angafunike thandizo la zacipatala . Ana adzafunika kukonza zokaonana ndi adokotala ndi kuthandiza makolo pa mbali zosiyana - siyana . Komabe , mabuku a zamalamulo a Aroma amakamba kuti zinali kucitikadi . YESU KHIRISTU Koma pamene ndinayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova , ndinazindikila kuti ndili ndi udindo wofunika kwambili wosamalila banja langa mwakuthupi ndi kuuzimu . Ubweya wopakidwa penti anaupeza m’mphanga lina pafupi ndi Nyanja Yakufa , ndipo unaonetsa deti la m’ma 135 C.E . Mphamvu yosaoneka yosintha anthu imene uthenga wa Ufumu uli nayo , imaonekela bwino m’maiko amene nchito ya Ufumu ndi yoletsedwa mwalamulo . Mumacitadi zimene mumaphunzitsa . ” Iyai . Ganizilani za Graham . Iye anacotsewa mu mpingo , ndipo pambuyo pobwezeletsedwa , anakhala wozilala . ( b ) Kodi mungalimbitse bwanji ubwenzi wanu ndi Yehova ? N’cifukwa ciani tingakambe kuti lamulo la Yesu limakhudza otsatila ake onse ? Ambili anali kudzaphedwa ndi lupanga , ndipo aliyense wopulumuka anali kudzatengeledwa ku ukapolo ku Babulo , nukakhala kumeneko umoyo wake wonse . ( Yer . GANIZILANI mmene zinthu zinalili cakumapeto kwa mwezi wa November mu 1932 ku Mexico City , mzinda umene unali ndi anthu oposa 1,000,000 panthawiyo . Koma ndale sizinalepheletse Mau a Mulungu kufikila anthu oona mtima . Anauzila Mfumu Davide kulemba kuti : “ Ndinali mwana , ndipo tsopano ndakula , koma sindinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa , kapena ana ake akupemphapempha cakudya . ” — Salimo 37 : 25 . Samalani kuti zitsanzo , mafanizo , kapena kakambidwe kanu , zisaphimbe mfundo za m’Baibo Baibo imati Mulungu ‘ anakhazikitsa dziko lapansi pamaziko olimba . Silidzagwedezeka mpaka kalekale , mpaka muyaya . ’ Monga mtumiki wacicepele wa Yehova , kapena wophunzila za iye , tidziŵa kuti iwe umakhulupilila mwa Mlengi . Koma kodi nthawi zina , umakhumbila zimene anzako ambili amakhulupilila , monga ciphunzitso ca cisanduliko ? Alendo okhalitsa : M’nthawi zakale , kuceleza kunali kuphatikizapo kukonzela alendo malo ogona . Anali masomphenya owopsa kwambili . Ndinali kulalikila m’ndende ndiponso kugaŵila mathilakiti kwa anthu amene ndinawapeza m’zimbudzi za pa malo ocezela . Imeneyi inali nchito yovuta , cifukwa kuti agaye mbeu anali kupela pamphelo . Ndipo mwina anali kusinja mu mtondo . Mau akuti “ mbeu , ” ayenela kuti anali atanthauzo kwambili kwa Abulahamu . Motelo , Yesu anacititsa kuti mbadwa za Adamu zikhale ndi moyo wosatha . Nanga n’zinthu ziti zimene nimakhulupilila kuti zidzacitika m’tsogolo ? 25 : 24 - 30 ; Luka 19 : 22 , 23 . Onani zina zimene salimo yaulosi imeneyi imakamba . Imati : “ Mwala umene omanga nyumba anaukana wakhala mwala wofunika kwambili wapakona . ” — Sal . Onani mmene io anali kucitila zimenezi . Ngati mwakhala m’banja kwa zaka zambili , muyenela kukhala citsanzo cabwino kwa acinyamata amene ali pabanja . 6 : 19 - 21 ) Dzifunseni kuti : ‘ Kodi ndili ndi mzimu wofanana ndi amuna amenewo ? Kuonjezela pamenepo , tingaphunzilenso njila zina zimene tingagwilitsile nchito pofotokozela ena zikhulupililo zathu mu utumiki . Conco , pokambilana ndi munthu mmene moyo unayambila , ni bwino kum’funsako mafunso coyamba . Ndipo zakudya zinam’cepela cakuti anapempha mkate kuti iye ndi anthu ake adye . ( 1 Sam . Kodi mumasinkhasinkha nthawi iti ? Anthu ambili masiku ano asokonezedwa ndi zimene zikucitika m’dzikoli kapena cifukwa cofuna - funa zinthu zakuthupi . Iye ndi woyenela kukhala mfumu cifukwa cakuti Mulungu ‘ ndiye mpando wake wacifumu . ’ Nsanja ya Mlonda yokhala ndi cingelezi cosavuta inayamba kufalitsidwa mu July 2011 . Ana amene amakonda Mulungu woona ndi kutsatila malamulo ake , amatonthoza ndi kulimbikitsa ena m’banja . Sitepi yoyamba ni kum’fikila Yehova mwa pemphelo locokela pansi pamtima . 8 : 3 ) Ndipo akanatsatila citsogozo ca Yehova , io akanapitiliza kukhala ndi umoyo wabwino . Aisiraeli analibe gulu lankhondo lamphamvu komanso analibe zida zankhondo zokwanila . Iwonso anali kum’dziŵa cifukwa anali mkazi wokongola maningi . Titalalikila ku zisumbu zimenezi kwa zaka 5 , tinayamba ulendo wopita ku Puerto Rico kuti tikasinthitse boti yathu ndi boti ya injini . Luka 21 : 11 : “ Kudzakhala zivomezi zazikulu . ” Mudzakhala “ Ufumu wa Ansembe ” Maganizo amenewa anali olakwika kwambili . Ngati timayang’anabe kwa Yehova , tidzaonetsa kuti timamulemekeza mwa kusiila malo mkwiyo wake ndi kumuyembekezela moleza mtima kuti adzacitepo kanthu pa nthawi yake yoyenela . Mau amenewa ni olingana kwambili na uphungu wa m’Baibo umene unalembewa zaka pafupi - fupi 2000 zapitazo , wakuti : “ Pakuti kukonda ndalama ndi muzu wa zopweteka za mtundu uliwonse , ndipo pokulitsa cikondi cimeneci , ena . . . adzibweletsela zopweteka zambili pathupi lawo . ” Oŵelengela ndalama m’kacisi sakanadziŵa kuti tumakobidi tuŵili tumenetu ndi amene anatupeleka , anali amtengo wapatali kwa Yehova . * ( Num . 27 : 14 ) Mulimonse mmene zinakhalila , cimene tidziŵa n’cakuti zimene Mose anacita zinapangitsa kuti Yehova asapatsidwe ulemu womuyenelela . Kodi munthu akatiitanila ku cakudya tifunika kucita ciani ? Mwina mumacitapo kanthu mwamsanga kuti mukonze zinthu . Iye anali monga “ mayi woyamwitsa ” kwa Akhristu a mumpingo wa ku Tesalonika . Pamene Ahabu anauza Naboti kuti am’gulitse munda wake wa mpesa , kapena kuti Ahabu atenge mundawo ndi kum’patsa munda wina wabwino kwambili , Naboti anakana . Akatswili amakamba kuti ndiye cifukwa cake maboma sangakwanitse kuthetsa ziphuphu . NYIMBO : 83 , 52 Conco , tingakambe kuti fanizo la Yesu likunena za masiku otsiliza ndi kuti adzabwela panthawi ya cisautso cacikulu . ( Luka 12 : 32 ; 1 Akorinto 15 : 49 , 50 ) Anthu amene adzaukitsidwila kumwamba adzalamulila dziko lapansi limodzi ndi Yesu . — Ŵelengani Chivumbulutso 5 : 9 , 10 . Woumba Wamkulu , Yehova , amathandiza anthu amene afuna kuumbidwa . Kodi kutsatila Khalidwe Lopambana kungatithandize bwanji kulemekeza nthawi ya anthu amene timakambilana nao ? Nanga bwanji za aja amene mwadala amakana kusintha njila zao ndipo amangopitilizabe kucita zinthu zoipa ? Cimodzi mwa zinthu zimenezi ndi kulalikila kunyumba ndi nyumba ndiponso mwamwai . Kodi kukhala ndi zolinga zakuuzimu kungatithandize bwanji kukonzekela dziko la tsopano limene Mulungu watilonjeza ? Iwo anamukwiyitsa ndipo Mose anayamba kulankhula mosalingalila bwino . ” Wina anali wopelekela cikho wa mfumu Farao ndipo wina anali wophika mkate . — Genesis 40 : 1 - 3 . Kodi mungatsanzile bwanji Elisa masiku ano ? N’zinthu ziti zimene munthu ayenela kusinkha - sinkha pa tsiku la ubatizo wake ? Iwo anakulila mumzinda umenewo , umene munali anthu olambila mafano ndi a makhalidwe onyansa , cakuti tsiku lililonse anali kufunika kucita khama kuti apewe makhalidwe oipawo . Kodi fanizo limeneli litanthauza ciani ? Iwo anamupezela thilansipoti ndiponso anamusankhila gawo limene angathe kulalikila mosavuta . Anali kuopa kucotsedwa pa udindo ndi kudzicotsela ulemu . Ndipo cidzakhala copepuka kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova popeza mwapang’onopang’ono tidzayamba kukhala angwilo . — Sal . Pamene anali kubwelako , Arthur anamvela anthu m’holoyo akuomba m’manja mwamphamvu ndi mwacikondwelelo . Kodi tingakhale “ oceleza ” m’njila ziti ? Munthu amene ali na cidziŵitso amadziŵa mfundo zambili . Conco , ine ndi Gwen tinayamba kuphunzila Baibulo ndi Gael ndiponso mwamuna wake Derrick . Mwacionekele , io sayang’ana kukula kwa cipatso kapena kutsika mtengo kwa cipatsoco . N’zinthu ziti zimene mungacite kuti mukhazikitse mtendele ? N’cifukwa ciani odzozedwa amachedwa “ mwana wamkazi wa mfumu ” ? Nanga n’cifukwa ciani akulangizidwa kuti ‘ aiwale anthu ao ’ ? ( Yes . 55 : 10 , 11 ) Ndipo zinthu zocititsa cidwi zimene zakhala zikucitika kwa zaka 100 zapitazi , zimaonetsa kuti Yehova ndi Mfumu . Munthu wina wochedwa Esibaala amachulidwa m’Baibo . Iye anali mmodzi wa ana a Mfumu Sauli . Ndiponso , angadziŵitse ana a makolowo zinthu zofunika monga makalata amene sanaŵelengedwe kapena mankhwala amene sanamwedwe . Mau olimbikitsa amenewa anathandiza Brian ndi Michelle kupitiliza ndi utumiki wao . Anali kukhululukila macimo ao ndipo sanali kuwaononga . 4 : 23 , 24 ) Ife tonse Akhristu tifunika kupitiliza kuvala umunthu watsopano ndi kusauvulanso mpaka pamene tidzakhala angwilo . Tiyeni tiyelekezele kuti tikuona m’maganizo mwathu zimene zinacitika pa nthawiyo . Akamayang’ana anthu kucokela pa malo ake okwezeka , mitundu yonse “ ili ngati dontho la madzi locokela mumtsuko , ndipo kwa iye ili ngati fumbi pasikelo . ” Ngati umu ni mmene zinthu zilili kwa imwe , tikukuyamikilani ngako cifukwa ca mzimu wanu wopilila . Chimo la Akani litaululika , Yoswa anamuuza kuti Yehova adzam’bweletsela tsoka . Cheyamani analengeza kuti m’cigaŵo cimeneci , aliyense ni wololedwa kutuluka m’holoyo , koma palibe amene adzaloledwa kungenanso . Amenewa angaphatikizepo kupatsa ena ulemu m’zinthu zing’ono - zing’ono monga kukamba kuti “ conde , ” na “ zikomo , ” komanso kuganizila ena . Masiku ano ambili alibe khalidwe limeneli , ndipo amaona zipangizo kukhala zofunika kuposa anthu . Komabe , Yehova amasangalala tikakhala oona mtima . M’nthawi ya atumwi , pamene Aroma anacoka ku Yerusalemu , sikuti inali nthawi yakuti Ayuda ambili atembenukile ku Cikristu . Mwacitsanzo , madzulo , pa machanelo ambili a TV pamakhala mapulogalamu oipa . ( Aheberi 11 : 8 , 11 , 15 ) Abulahamu na Sara sanaganizilepo zimene anasiya kumbuyo . 96,206 Lemba la Aroma 5 : 12 limati : “ Ucimo unaloŵela m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi , ndi imfa kudzela mwa ucimo , imfayo n’kufalikila kwa anthu onse cifukwa onse anacimwa . ” 46 : 6 , 7 . 5 : 14 . Mkulu wina amene watumikila zaka zambili m’dziko lina losauka anati : “ Nthawi zambili anthu amanena kuti Mboni za Yehova ndi anthu acimwemwe . ( Yobu 1 : 13 - 19 ) Kenako Satana anacititsa Yobu kudwala matenda opweteka ndi onyansa . Koma Gidiyoni mwakabisila anali kupuntha tiligu m’nkhuti kuti Amidyani asauone . Monga mmene Yesu anakambila , sitikudziŵa tsiku leni - leni kapena ola pamene mapeto adzafika . N’cifukwa ciani kupitilizabe kuonetsa cikondi n’kofunika ? 2 : 18 - 23 . ( b ) Nanga ena apindula bwanji posinkhasinkha pa zimene aŵelenga ? Uthenga wabwino ndi wakuti sitifunika kudalila anthu kuti ndi amene angathetse imfa . ( Mateyu 5 : 3 ) Iye amatipatsa “ zinthu zonse kuti tisangalale . ” Mwina zimene amatilakwilazo zingakhale zazing’ono , koma tikawakhululukila timaonetsa kuti timawakonda . Tidzakhala ofunitsitsa kulamulidwa ndi Yehova , amene ndiye woyenela kulamulila ndipo amalamulila mwacikondi . Yoswa , mthandizi wa Mose , anafuna kuwaletsa . Nanga bwanji ponena za mafanizo ena amene Yesu anafotokoza mwatsatanetsatane ? Ndipo padzikoli pali maiko ambili amene ciŵelengelo ca anthu m’dziko lililonse palokha n’cocepa poyelekezela ndi ciŵelengelo ca anthu onse a Yehova . Kodi kudalila Yehova kungatithandize bwanji pankhani ya ufulu wathu ? Patsiku limenelo , mkulu wa ansembe anali kutenga magazi ansembe zanyama , ndi kuloŵa nao m’Malo Oyela Koposa m’cihema . N’ciani cinacitikila Terofimo ndi Epafurodito ? Nanga zimenezi zitiphunzitsa ciani ? Kulela ana “ m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake ” ni udindo umodzi waukulu umene kholo lililonse lacikhristu lili nawo . Nanga n’cifukwa ciani sanacite zimenezo ? ’ Tingakhale na mtendele wa m’maganizo ngati tisamalila ‘ zosoŵa zathu zauzimu . ’ — Mateyu 5 : 3 . Yesu anaonetsa kuti anali wozindikila m’mau ndi zocita zake . Iye anapatsidwanso lupanga lalikulu . ” — Chivumbulutso 6 : 4 . Pa Mateyu caputala 5 mpaka 7 , Yesu anagwilitsila nchito mau omveka bwino kwambili . Filip anati : “ Pamene mwayi unapezeka , tinali kumvela monga Yehova akutiuza kuti ‘ Lomba mungapite . ’ ” A Zulu : Mwacidule tiyeni tibweleze zimene takambilana . Ngakhale m’maiko amene mulibe ziletso , uthenga wa Ufumu umafika ku madela akutali kumene Mboni zakumaloko zimaona kuti n’zosatheka kufikako . Nanga kudziŵa zimenezi kungalimbitse bwanji cikhulupililo canu cakuti akufa adzauka m’tsogolo ? 4 : 20 ) Kuwonjezela apo , kukonda Yehova ndi abale athu , kumagwilizana ndi kukonda Baibo . 17 : 14 ; 19 : 19 ) Kodi kuukila kumeneku ndi kosiyana ? Conco , kwa Mulungu Adamu ndi Hava anafa tsiku limene anacimwa , ndipo io anafa “ tsiku ” lisanathe , limene ndi zaka 1,000 . — 2 Pet . Tiyenela kuyesetsa kulimbana ndi zofooka zathu podziŵa kuti zimenezi zidzakondweletsa Yehova . Kodi tingatsanzile bwanji mtima wake wodzipeleka ? Conco , pafupi - fupi munthu aliyense , kuphatikizapo aja amene amadziŵa Ciheberi na Cigiriki camakono , amafunika kuŵelenga Baibo yomasulilidwa kuti amvetsetse Mau a Mulungu . Iye anati : “ N’nadzimva kukhala munthu wopanda pake , n’nalibenso mwana , n’nalibenso nyumba , n’nalibenso mwamuna . Anthu amakula mosiyana - siyana . Kunena zoona , munthu wopatsa amalimbikitsa cikondi ndipo anthu ena amasangalala kukhala naye . Lamulo la Aroma linali kugwila nchito mu ufumu wonsewo , ndipo anthu amene anali nzika za Roma anali kupatsidwa ufulu ndiponso kutetezedwa . Yesu anauza omvela ake kuti : “ Ine ndine cakudya copatsa moyo . Aisiraeli sanayamikile ufulu umene Yehova anawapatsa mwa kuwatulutsa mu ukapolo ku Iguputo . ( Mateyu 11 : 19 ) Kodi simukuvomeleza zimenezi ? Mbali yaciŵili inakhudza kusokonezedwa kwa ulamulilo wa Mulungu . Zitiphunzitsa kuti Baibulo ili ndi mphamvu zotha kusintha anthu ; inde , kusintha kaganizidwe kawo . ( b ) Ni fanizo iti imene tidzakambilana ? Cifukwa ? Kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova kungatithandize kupewa ciwelewele . Conco , tiyenela kukonda Yehova ndi moyo wathu wonse kuphatikizapo zonse zimene tili nazo . Ni mbali ziti za kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu zimene tiyenela kuuzako ena ? Koma timawalemekeza ndi kuwamvela mogwilizana ndi mfundo za m’Malemba . Mzimu woyela wathandiza Bungwe Lolamulila kumvetsa bwino coonadi ca m’Malemba cimene sanali kucimvetsa poyamba . Conco , munthu akazoloŵela kukoka amakhala ndi mavuto ena cifukwa coleka kukoka . Masiku ano , anthu mamiliyoni ambili amalambila Yehova . Iwo na mtima wonse amaseŵenzetsa ‘ zinthu zawo zamtengo wapatali , ’ monga nthawi yawo , mphamvu , na cuma cawo , pocilikiza nchito yomanga kacisi wamkulu wauzimu wa Yehova . ( Miy . 3 N’cifukwa Ciani Mufunika Kuŵelenga Baibo ? Zimenezi n’zolimbikitsa . “ Mau a Mulungu ndi amoyo . ” — AHEBERI 4 : 12 . Pamene nkhope ya wopelekela cikho inaoneka kuti yamasuka , Yosefe anamupempha kuti : “ Conde , udzandikomele mtima pondichula kwa Farao . ” George Rollston ndi Arthur Willis amene ni apainiya aima pang’ono kuti athile madzi mu injini ya motoka . — Ku Northern Territory , 1933 Kodi pamakhala zotulukapo zanji ngati munthu amakonda Mulungu ? Kuwonjezela apo , umboni wozikidwa pa zinthu zakale uonetsa kuti zinali zofala kwa mafumu aciiguputo kulanda mkazi wamwini mwacikakamizo na kupha mwamuna wake . Malo acete ndiponso oyenelela amathandiza anthu kuphunzila ndi kukambilana zinthu zakuuzimu bwinobwino . 65 : 12 - 14 ) Yehova amalemekezedwa ngati anthu ake apanga zosankha mwanzelu pa umoyo wawo . — Miy . ( b ) Kodi Mulungu amayankha bwanji mapemphelo athu ? Kodi Paulo anacenjeza Akhristu anzake pa zinthu ziti ? Kodi Yehova watiphunzitsa bwanji kuti tizim’konda ? Ngakhale kuti Davide anacitapo macimo , anali munthu wokonda Yehova , wodzipeleka pa kulambila koona , ndipo analapa macimo ake na mtima wonse . — 1 Maf . Nanga n’ciani cinam’thandiza kukhalabe wodzicepetsa ? Mosakaikila , anthu aŵili amenewa anakhala paubwenzi wolimba . Iwo anali kulimbikitsana , ndipo kucita zimenezi kunawathandiza kuti asataye mtima ndi zinthu zambili zopanda cilungamo zimene anali kuona m’dzikolo . N’zoonekelatu kuti Yehova anali kuwatsogolela . Conco , Davide anam’konzela ciwembu kuti akaphedwe ku nkhondo . Anafunika kutsogolela mtundu wa Aisiraeli kukaloŵa m’Dziko Lolonjezedwa , ndipo anali kuyembekezela kukumana na adani oopsa . Kenako , io anali kuzitumiza kwa olemba manyuzipepala a ku Canada , Europe , ndi ku United States . Ndithudi uzitsatila cilungamo . ” M’malo motifotokozela zinthu za kumwamba m’njila imene sitingamvetsetse , Mulungu anaonetsa atumiki ake masomphenya a zinthu zakumwamba m’njila yosavuta kumva . Kodi abale atatu amene akhala akugwila nchito ndi a m’Bungwe Lolamulila anakamba ciani ? Ndipo zimene anakamba zingakuthandizeni bwanji kukhala oyela ? Mfundo imeneyo inatithandiza kuona kuti tikhoza kusintha zolinga zathu zauzimu . ” 2 , 3 . ( a ) Kodi maganizo akuti Satana kulibe amamuthandiza bwanji kukwanilitsa zolinga zake ? Sitinadziŵe kuti dziko la Ireland lisiyana bwanji ndi dziko la England . Ndiye cifukwa cake kuimba , kaya patekha kapena pamodzi na anthu a Mulungu , ni mbali yofunika ngako pa kulambila koona . Mofananamo , mitu ya mabanja ndi akulu amene amakonda ulamulilo wa Mulungu sacita kukakamiza anthu kuwamvela , monga kuti anakhazikitsa kaulamulilo kawo . Tikatelo , ndiye kuti tikutengela Atate wathu wacikondi ndi wacifundo , Yehova . — Sal . Ena angapeze basi maganizo awo ali pa kukonda kumwako mitundu yosiyana - siyana ya moŵa kapena waini , kaya kutengeka kwambili na kukongoletsa pa nyumba , kugula zovala zili m’fashoni , kupeza njila zopezela ndalama , kukonza zokayenda pa maholide , na zina zaconco . Palibe mphatso yocokela kwa munthu waudindo , kapena imene inapelekedwa cifukwa ca cikondi cacikulu imene ingapose nsembe ya Yesu . Mwiisiraeli wina anali atanyozapo Mose kuti : “ Anakuika iwe ndani kukhala kalonga ndi woweluza wathu ? ” ( Eks . MMENE TINGAONETSELE KUTI TIMAM’KONDA MULUNGU Conco , ‘ citamponi kanthu kuti mucipeze ’ mwa “ kufufuza Malemba mosamala ” ndi mwakhama tsiku ndi tsiku . — Mac . 17 : 11 . Tinali kufuna kupitilizabe utumiki wa nthawi zonse , ndipo tinali okonzeka kucita utumiki uliwonse . ( b ) Nanga Yesu anawathandiza bwanji kuwongolela maganizo awo ? Vuto lina linali kuuzako ena za cikhulupililo canga pocita ulaliki wa ku nyumba ndi nyumba . Rebecca anati : “ Tinaona kuti Yehova sanatisiye . Mosiyana ndi m’bale John na mlongo Judith , ena amakwanitsa kucita upainiya kwa nthawi yocepa cabe . N’cifukwa ciani anthu a Mulungu anali na ciyembekezo cakuti adzamasuka mu ukapolo kwa Babulo ? Nanga tikambilana mafunso ati ? Ndikukaikila ngati kuli munthu wokhulupilika m’banja kapena amene amafuna kutelo . ” Conco , zocitika zapadela zimene takambilanazi zinathandiza kuti nchito yolalikila uthenga wabwino iyende bwino . Kodi munadzipeleka kwa Yehova ndi kuonetsa kudzipelekako mwa kubatizika m’madzi ? Ni malangizo ena ati a m’Baibo amene amatipindulitsa ? Iye anapatsa Sisera malo kuti apumule . Tili ndi moyo cifukwa cakuti Nowa anatsatila malangizowo mosamalitsa . — Gen . Tingaphunzilepo ciani pamenepa ? Kumeneko , anawavula malaya awo akunja mocita kuwang’ambila ndi kuwakwapula na zikoti . ( Mac . 16 : 16 - 22 ) Ha ! Kodi Yehova anaika ciani m’dzanja la Mose ? 4 : 10 ) Iwo anasintha kaganizidwe kawo , olo kuti kucita zimenezi kunawatengela nthawi . 4 : 2 ) Kodi inunso mudzayesetsa kucita zimenezi kuti mulimbikitse mtendele ? Kucita zimenezi n’kupanda cikondi . 6 : 1 - 5 ) Kugaŵila cakudya catsiku ndi tsiku kunali makonzedwa akanthawi . Makonzedwe amenewa anali akuti asamalile zosoŵa za anthu amene anakhala Akristu pa Pentekosite mu 33 C.E . 61 : 1 , 2 ; Luka 4 : 18 - 21 . Iye ndi Tate wabwino koposa . Kutumikila Yehova mwakhama kumatithandiza kuika maganizo athu pa malonjezo a mtsogolo . ( Ezara 2 : 58 , 64 , 65 ; Estere 8 : 17 ) Masiku ano , a “ khamu lalikulu ” la “ nkhosa zina ” za Yesu , amacilikiza mokhulupilika Akristu odzozedwa amene ndi “ Isiraeli wa Mulungu . ” ( Chiv . 7 : 9 , 10 ; Yoh . 10 : 16 ; Agal . Kodi Yehova anam’thandiza bwanji Mose kuti akwanilitse utumiki wake ? F . Ena adzasangalala kukhala mafumu ndi Kristu kumwamba , ndipo ena adzakhala padziko lapansi monga nzika za Ufumu wa Mulungu . Kodi ndinu wokonzeka kutsatila malingalilo awa ? Akhristu a m’nthawi ya atumwi sanalole tsankho kusokoneza mgwilizano wawo . Koma cimeneci siciyenela kukhala cifukwa cacikulu cokhalila wacifundo . Malonjezo a Mulungu ali monga mankhwala ozizilitsa ululu wa nkhawa zathu . Ganizilani citsanzo ca mlongo wina dzina lake Mirjeta * amene amakhala ku dziko limene poyamba linali Yugoslavia . Baibulo limati : “ Inu akazi , muzigonjela amuna anu , pakuti zimenezi ndiye zoyenela kwa anthu otsatila Ambuye . ” ( Akol . N’cifukwa ciani acicepele amene tili nawo mu mpingo timafunika kuwayamikila kwambili ? Khalani “ olimba mtima . ” Kodi kukonda abale athu kumabweletsa madalitso anji ? N’zoona kuti m’dongosolo lino la zinthu sitingathetse maganizo onse olakwika kapena zofooketsa . Kugwila nchito yopanga ophunzila kungakuphunzitseni kukhala akhama pa nchito , kukhala na luso lokamba bwino ndi anthu , kugwila nchito na mtima wonse , ndi kukhala wozindikila . ( Miy . 21 : 5 ; 2 Tim . Yelekezelani kuti ziwalo za thupi lanu ndi zakufa kupatulapo maso . Kodi Yehova amapeleka motani malangizo kwa atumiki ake ? Mwacitsanzo , m’kalata yake yaciŵili yopita kwa Akhristu a ku Korinto , iye anati : “ Yehova ndiye Mzimu , ndipo pamene pali mzimu wa Yehova , pali ufulu . ” — 2 Akor . Yesu atangobatizika , anayamba nchito imene inali kudzafalikila padziko lonse lapansi . Mzimu wa Mulungu umacitila umboni ndi mzimu wao kuti ndi ana odzozedwa a Yehova . Ndi thandizo la Yehova , pezani njila za mmene mungapangile utumiki wanu kukhala wokhutilitsa ndiponso waphindu . Boti yochedwa Sibia tinaiseŵenzetsa monga nyumba kucokela mu 1948 mpaka 1953 ( kulamanja ) Ngakhale masiku ano , ciwembu ca m’cikwati sicingaloledwe pakati pa anthu a Yehova . Pangano limene Yehova anacita ndi Abulahamu linayamba kugwila nchito pa Nisani 14 , 1943 B.C.E . Angafuule kwa Yehova cifukwa ca zimene iweyo wam’citila , iwe n’kupezeka kuti wacimwa . ” Baibo imati : “ Pali kumwamba kwatsopano ndi dziko lapansi latsopano zimene ife tikuyembekezela mogwilizana ndi lonjezo lake , ndipo mmenemo mudzakhala cilungamo . ” — 2 Petulo 3 : 13 Olo kuti zinali conco , nkhawa yaikulu ya Yefita siinali pa zimene tachulazi . Pa msonkhano wina wapadela , Herode anavala “ zovala zake zacifumu . ” ( 1 Sam . 8 : 5 ) Ngakhale zinali conco , Yehova ndi amene anali Mfumu yao ndipo mfundo imeneyi inaonekela bwino pamene Davide , mfumu yaciŵili ya Isiraeli anali kulamulila . Ndalama zimaimila udindo wa mtengo wapatali wophunzitsa anthu kukhala ophunzila . Mofananamo , anthu okhulupilila Yehova angadalile “ mphamvu yoposa ya cibadwa ” imene iye amawalonjeza . — 2 Akorinto 4 : 7 , 8 . Adzakhala wosangalala kuona mmene nchito yake yapindulitsila abale ndi alongo mumpingo . ( Ŵelengani Mateyu 22 : 16 - 18 . ) Komabe , Yehova amakondwela kwambili ngati tigwilitsila nchito nthawi yathu mwanzelu mwa kuŵelenga ndi kuphunzila Baibulo ndi zofalitsa zathu . NYIMBO : 123 , 53 Koma kukhala oona mtima pa zinthu zimene zingakuonetseni monga kuti ndimwe wolakwa , ndiye kumapangitsa kuti anthu akudalileni kwambili . ” — Caiman . 43 : 10 ) Timapempha Atate wathu wa kumwamba kuti : “ Dzina lanu liyeletsedwe . ” 14 : 7 ) Ino ndiyo nthawi yolengeza uthenga umenewo . ( Gen . 15 : 6 ) Iye anaika maganizo ake pa zinthu zakumwamba mwa njila yakuti anali kuganizila za malonjezo a Mulungu . Zotsatilapo zake n’zakuti Mulungu Wam’mwambamwamba anam’dalitsa . Nthawi zambili , anali kuletsa anthu kukhala ndi Baibulo , kuisindikiza , kapena kuimasulila . Baibulo Lomasulidwa Bwino Kwambili ( Yak . 2 : 8 ) Pambuyo pochula malamulo ena a m’Cilamulo ca Mose , Paulo anati : “ Lamulo lina lililonse limene lilipo , cidule cake cili m’mau awa akuti , “ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ” Nthawi zina , si bwino kufalitsa nkhani ngakhale kuti ndi yoona . Koma anthu akuthupi ni zitsanzo zoticenjeza . ( 1 Akor . Zimene wansembe wocita za mayele uja anakamba zinali zosoceletsa ndiponso zopanda phindu . Kuti mudziŵe maulosi ena a m’Baibulo okhudza Mesiya ndi mmene anakwanilitsidwila , onani patsamba 200 m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceniceni . Ife tonse ndife ocimwa , conco tinali oyenelela kufa . ( Sal . Omasulila Baibulo la Dziko Latsopano m’zinenelo zosiyanasiyana zoposa 130 , akhala akutsatila mfundo zitatu zimenezi . Ndipo timawalimbikitsanso mwa kupeleka mayankho ndi kuimba nyimbo mocokela pansi pamtima . — Akolose 3 : 16 . Tonsefe tingathandize kuti munthu wocotsedwa apindule ndi cilango cimene wapatsidwa . Akristu amenewa anganene kuti mzimu “ umacitila umboni , ” kapena kuti umawatsimikizila kuti adzalandila mphoto yakumwamba 7 : 8 , 9 . ( Sal . 51 : 17 ) Pamene Akhiristu a ku Tesalonika anali kuzunzidwa , Paulo anawalembela kalata ndi kuwauza kuti : “ Ambuye wathu Yesu Khristu mwiniyo , ndi Mulungu Atate wathu , amene anatikonda ndipo amatilimbikitsa m’njila yosalephela ndiponso anatipatsa ciyembekezo cabwino , mwa kukoma mtima kwakukulu , alimbikitse mitima yanu ndi kukulimbikitsani . ” ( 2 Ates . Kodi mkwatibwi wake ndani ? 119 : 116 ) Luis , katswili wopanga makina ozimitsila moto , ndi mkazi wake Quenia akutumikila ku Wallkill . Tsiku lina azimai aŵili a Mboni za Yehova anabwela kudzagula zipatso . Iye anati : “ Nimadzimva kuti ndine womasuka ku mkwiyo umene unali utaononga umoyo wanga . Tunsimbi tumeneto anali kutupinda kuti tuzikwana bwino pa thupi la msilikali , ndipo anali kutumanga na nthambo za cikumba . Patapita nthawi , anthu ena otumidwa na mtundu wa Isiraeli anapita kwa iye na kum’dandaulila kuti : “ Bambo anu anaumitsa goli lathu . Ethel Bennecoff anakamba kuti pamene Ophunzila Baibulo anabwelela kumanyumba kwawo , ‘ cangu na cikondi [ cawo ] zinawonjezeka kwambili . ’ ( 5 ) Kusacita mantha . Koma ndinadziŵa kuti Yehova anapatsa ine ndi mwamuna wanga udindo wolela mwana . ” Mwacitsanzo , pamene M’bale Edwin Skinner anafika ku India mu 1926 , m’dzikolo munali Mboni zocepa kwambili . Iye analola zimene anaphunzila m’Baibo kumufika pamtima . Anthu anali pilingupilingu mumzindamo pamene anali kubwela kudzacita cikondwelelo capadela cimeneci . Kwa zaka , ine na amuna anga tinayamba taima kucita upainiya . Kupitila m’mabuku athu , atumiki a Yehova amalandila zakudya ndi zakumwa za kuuzimu zoculuka . ( Yes . Kuti mudziŵe mmene coonadi ca Ufumu casinthila maganizo ndi zocita za wophunzila , mungamufunse kuti , ‘ Kodi kudzipeleka kwanu kwa Yehova kwakhudza bwanji mmene mumagwilitsila nchito moyo wanu ? ’ Yefita anali mwamuna wamphamvu komanso wolimba mtima , ndipo mbili ya Aisiraeli anali kuidziŵa bwino kuphatikizapo Cilamulo ca Mose . ( 1 Akorinto 13 : 7 ) Ndipo sitiyenela kukhulupilila mabodza kapena zinthu zoipa zimene ena amakamba ponena za gulu la Yehova , komanso abale athu amene timakonda . Pokambilana , tidzaona zitsanzo zisanu za maganizo a dziko na mmene tingawapewele . Goliyati anatembelela Davide m’dzina la milungu ya Afilisiti ndipo analumbila kuti apeleka mnofu wake kwa mbalame zam’mlengalenga ndi kwa zilombo zakuchile . — 1 Samueli 17 : 41 - 44 . ( b ) N’cifukwa ciani kuyamikila wophunzila n’kofunika ? Kuti mutsimikize zimenezi , tsegulani Baibulo lanu ndi kuŵelenga Malemba awa : Salimo 37 : 9 - 11 ; 46 : 8 , 9 ; 72 : 7 , 8 , 16 ; Yesaya 35 : 5 , 6 ; 65 : 21 - 23 ; Mateyu 5 : 5 ; Yohane 5 : 28 , 29 ; Chivumbulutso 21 : 4 . Cinawathandizanso kucita malonda moona mtima , ndi kukomela ena mtima . ( Eks . 20 : 14 ; Lev . 19 : 18 , 35 - 37 ; Deut . A Robert anati : “ Ngati ndilola ana athu kucita zinthu zimene andipempha , kenako n’kudzazindikila kuti mkazi wanga anali atawaletsa kucita zinthuzo , ndimasintha maganizo kuti ndigwilizane naye . ” Ndipo iye anapeleka citsanzo cabwino kwambili ca cikhulupililo cimene ife tonse tifunika kutsanzila , kaya ndife acinyamata kapena acikulile . NYIMBO : 49 , 73 N’ciani cimene mungacite kuti muzionetsa kuwala kwanu kwa anthu okhala nawo pafupi ? Titamasulidwa , tinapitiliza kuyendela mipingo mwakabisila . 1 : 9 , 10 ) Cidziŵitso colondola cimeneco kapena kuti colongosoka , cikanathandiza Akhiristu a ku Kolose ‘ kuyenda mogwilizana ndi zimene Yehova amafuna , kuti azimukondweletsa pa ciliconse . ’ Nditafika zaka 12 , ku Spain kunabuka nkhondo yapaciŵeniŵeni . Kodi Abulahamu na banja lake anaika maganizo ake pa ciani ? Nanga n’ciani cinawathandiza kukhalabe na cikhulupililo colimba ? Ngakhale ngati zinali conco , nchito imene Yosefe na Nikodemo anagwila siinali yocepa . Johannes Kodi makolo afunika kucita ciani zikakhala conco ? Kuwonjezela apo , Boazi sanakambe mau ofooketsa kwa mkazi wacilendoyu , m’malo mwake anamulimbikitsa . — Rute 2 : 8 - 10 , 13 , 14 . 4 : 29 ) Komabe , ciyamikilo cathu ciyenela kukhala cocokela pansi pa mtima . Kodi munadzifunsapo mafunso otelewa ? Palibe cinthu coŵaŵa kuposa kusiyidwa na Mulungu . Zimenezo zinapangitsa kuti abale ake am’citile nsanje kwambili moti anamugulitsa ku ukapolo . — September - October , tsamba 11 - 13 . Mulungu anawacha kuti “ anthu anga amene ndawapanga kuti akhale anga , anene za ulemelelo wanga . ” Ndipo nkhani zokhudza zocita za anthu zoposa 60 za mutu wakuti “ Baibulo Limasintha Anthu , ” zafalitsidwa mu Nsanja ya Olonda kwa zaka zingapo tsopano . ZEKARIYA ayenela kuti anayamba kuganizila zambili pambuyo poona masomphenya a namba 7 . Koma lomba m’pamene ningakambe kuti nimam’kondadi Yehova . ’ Chati comwe anali kugwilitsila nchito poyendetsa zizindikilo za pa Cikumbutso ku holo yocedwa London Tabernacle ( Chivumbulutso 4 : 11 ) Kuonjezela pamenepo , tidziŵa kuti panthawi inayake cilengedwe kunalibe . Adamu ndi Hava anakana ulamulilo wa Yehova . Monga mmene Genesis caputa 3 imakambila , colinga ca Yehova cinasokonezeka . ( Gen . Kodi Abulahamu anadziimbapo mlandu cifukwa comvela malamulo a Yehova ? Monga mmene mitengo ya mpesa yobala zipatso zabwino imacititsila kuti mlimi alemekezeke , na ise tikamalalikila uthenga wa Ufumu mwakhama , timacititsa kuti Yehova alemekezeke na kupatsiwa ulemelelo . — Mat . Iye amawakumbukila bwino kwambili ndipo anati : “ Amenewo anali apainiya acangu , ofikilika , okoma mtima ndipo anali kulidziŵa bwino kwambili Baibulo . ” ( b ) Tikuphunzilapo ciani pa citsanzo ca Yosefe ? COLINGA : Kuyala maziko ovomelezeka a “ mbeu ” ya “ mkazi ” ya pa Genesis 3 : 15 kuti ikalamulile mu Ufumu Kutsanulila kwa mzimu kumeneku kunanenedwelatu ndi Yehova m’mau awa : “ Ndidzatsanulila mzimu wanga pa camoyo ciliconse , ndipo ana anu aamuna ndi ana anu aakazi adzanenela . . . . ( Ŵelengani Zekariya 6 : 15 . ) Tikaona zimene dipo yakwanilitsa , sitikaikila kuti mphatso ya dipo yocokela kwa Mulungu , imene yacititsa kuti tidzakhale na moyo wosatha , ndiye mphatso yopambana zonse . Pambuyo pokhala kapolo wa mankhwala osokoneza ubongo kwa zaka 30 , Alonso anayamba kuphunzila Baibo na Mboni za Yehova . ( 1 Timoteyo 3 : 2 , 11 ) Kukhala na cizoloŵezi ca kudya na kumwa kwambili kumaononga thanzi lathu komanso ndalama zathu . Ndiye cifukwa cake mtumwi Paulo anati : “ Kristu ndiye mphamvu ya Mulungu . ” ( 1 Akor . 7 : 35 ) Yehova anapeleka Cilamulo kupitila mwa angelo . Cilamuloco n’cimene Mose anaseŵenzetsa kulangiza Aisiraeli . ( Agal . 1 : 8 ) Poganizila mavuto amenewa , ophunzilawo ayenela kuti anakaikila ngati adzakwanitsa nchitoyo . Kulambila Baala kunali kofala m’dzikolo ndipo Eliya anafunika kucita zambili kuti athandize anthuwo . Khalani woyamikila Makolo , citsanzo canu n’cofunika kwambili kuti muthandize ana anu kuyamba kuyenda m’njila ya ku moyo wosatha . 12 Kutumikila Yehova ‘ m’Masiku Oipa ’ Kukhala wololela kungakuthandizeni kupewa kukangana pa zilizonse m’banja . — Afil . Conco , anaganiza zakuti am’thandize . Ndipo kukamba zoona , sin’nali kufuna kuti ticoke mu utumiki umenewo na kuyamba nchito yoyendela dela . Koma Yehova anali nase na colinga cinacake . ” Nthawi zambili ofalitsa amafikila anthu amene angocoka kumene kupempha thandizo kwa Mulungu . Pamene Yesu anali padziko lapansi , nchito yake yaikulu inali kulalikila uthenga wabwino . Nowa mwacitsanzo . Anali wokhulupilika ndipo anasankha kulabadila malangizo a Mulungu omanga cingalawa copulumutsilamo banja lake , kutinso kukabadwe mibadwo ina m’tsogolo . ( Aheb . Kukonda cuma . Conco , zotulukapo za umoyo wosadalila gulu la Mulungu na malangizo ake ni kupanda cimwemwe ndi mavuto ena ambili - mbili . Ena a io anabwelela kwao ku Poland kukaphunzitsako ena coonadi camtengo wapatali cimene anaphunzila . Baibo imati iye “ anacitadi momwemo , ” kutanthauza kuti anatsatila malangizo a Yehova . ( Gen . Baibulo limakamba kuti : “ Kenako , Gidiyoni anafika ku Yorodano n’kuwoloka mtsinjewo pamodzi ndi amuna 300 amene anali nao aja , ali otopa . ” Ndiye cifukwa cake tingakambe kuti mpingo Wacikristu unali kapolo wa Babulo Wamkulu . 104 : 1 , 2 . 1 , 2 . ( a ) Kodi m’busa waciisiraeli anali ndi maudindo otani ? Kukamba zoona , zidzakhala zosangalalatsa kwambili kukhala m’dziko limene onse adzakonda Yehova ndi anzao . 121 : 5 ) Anna anati : “ Panopa nili na cimwemwe coculuka kuposa kale lonse . Pangano limenelo linali losiyana ndi pangano la Cilamulo , cifukwa linacititsa kuti macimo akhululukidwe popanda kupeleka nsembe za nyama . Baibulo limakamba kuti : “ Amuna inu , pitilizani kukonda akazi anu monga mmene Kristu anakondela mpingo n’kudzipeleka yekha cifukwa ca mpingowo . ” ( 2 Akorinto 1 : 3 ) Onani njila zinayi zikulu - zikulu zimene Mulungu amaseŵenzetsa potonthoza anthu . Kodi ni malonjezo ati amene adzakwanilitsidwa mu Ufumu wa Mulungu ? ( Sal . 133 : 1 ) Kuwonjezela apo , Mau a Mulungu amakamba kuti Yehova amateteza anthu ake kwa Satana na ziŵanda zake . ( Sal . Kaya moyo wathu ukhale pangozi , sitidzagonja kwa anthu amene sadziŵa Yehova amene angatikakamize kuti tisamvele Mulungu . Mulungu amatiuza kuti : “ Ine sindisangalala ndi imfa ya munthu woipa , koma ndimafuna kuti munthu woipa abwelele kusiya njila zake n’kukhala ndi moyo . ” — Ezek . ( Eks . 1 : 13 , 14 ; Mac . 8 : 28 - 32 ; Yoh . 2 : 13 - 17 ; 18 : 3 - 5 ) Citsanzo cake cinawathandiza kukhala olimba mtima . Bulletin inayamba kuchedwa kuti Informant . Koma masiku ano , imachedwa kuti Utumiki Wathu wa Ufumu . Kodi Yehova angatitonthoze bwanji ? Mwacitsanzo , mapemphelo ao angathandize kuti mpingo ulimbe mwa kuuzimu . — Ŵelengani Salimo 92 : 13 , 14 . Antoine ndi mmodzi wa ana amene anabadwa kwa anthu a ku Poland ca m’ma 1920 ndi 1930 . N’cifukwa ciani kulola ena kutipangila zosankha kungakhale koopsa ? Koma anthu ambili anakana Yehova kuti akhale Atate wao ndi Mfumu yao . Ndipo sipadzakhalanso munthu wofunsa kuti , ‘ Kodi imfa ndi mapeto a zonse ? ’ Muziganizila kwambili za madalitso amene mudzalandila . Mudzakhala osangalala , cikondi canu pa Yehova cidzalimba , ndipo mudzamuyandikila kwambili . — Yak . Mkhristu waconco afunika kupeza nchito ina . Coyamba , ganizilani cimene cimakucititsani kukhutila na zimene mumakhulupilila . Kukhala ndi “ cifundo cacikulu ” ndi mbali ya umunthu watsopano umene Akristu onse ayenela kuvala . Angakhalenso kuti sadziŵa citundu kapena cikhalidwe ca kwanuko . Conco , mungawaitanileko ku nyumba kwanu kuti mudzadye nawo cakudya , kapena mungawapemphe kuti mukayende nawo kwina kwake . Ndipo mzela wobadwila wa Yesu unali wodziŵika ngako cakuti ngakhale Afalisi ndi Asaduki sanatsutse za mzelawo . 32 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi Yehova amaona mbali imene tingam’tumikile bwino kwambili . ( Yuda 6 ; 2 Petulo 2 : 4 ) Ziŵanda zimenezo zinagwilizana ndi Satana Mdyelekezi “ wolamulila ziŵanda , ” amene “ amadzisandutsa mngelo wa kuwala . ” — Mateyu 12 : 24 ; 2 Akorinto 11 : 14 . Tinali kusinthana - sinthana pocita mbali za misonkhano , wina atsogoza wina ayankha mafunso . Nthawi zina , Mulungu angalole kuti tikumane ndi vuto linalake , kuti tionetse cikhulupililo cathu mwa iye . Kenako . . . ulemelelo wa Yehova unadzaza nyumba ya Mulungu woona . ” Idzatithandizanso kudzipenda ndi kuona mmene ise patekha , timaonela utumiki wopulumutsa moyo umene Akhristufe tinapatsidwa , ndi coonadi cimene takhala tikuphunzila zaka zonsezi . Pasanapite nthawi , Tessie anayamba kufika pamisonkhano ndipo anayamba kuonetsa makhalidwe acikhiristu ngakhale kuti mabwenzi ake akale anali kumuseka . Koma kodi anthu onse amene ali m’zipembedzo za Babulo Wamkulu adzaphedwa pamene zipembedzo zimenezi zidzaonongedwa ? Ndithudi , iye n’citsanzo cabwino kwambili kwa aliyense wa ife . — Mlaliki 12 : 1 6 : 17 ) Komanso pambuyo pokhala Mboni ya Yehova , mlongo uja wa ku Central Europe , anakwatiwa na m’bale wa mtundu umene anali kudana nawo poyamba . Mosiyana ndi kale lonse , anthu mamiliyoni ambili amitundu yonse akutsatila kulambila koona . Nthawi zina tingathedwe nzelu ndi mavuto athu , koma tiyenela kukumbukila kuti palibe vuto limene Yehova angalephele kuthetsa cifukwa ali ndi mphamvu zopanda malile . Tinaimilila ndipo m’maso mwathu munadzala misozi yacisangalalo . ” Sukuluyi imacitika m’mipingo yoposa 111,000 padziko lonse lapansi . Mfundo imeneyi imagwilanso nchito kwa aja amene amakamba kuti amalambila Mulungu koma mwadala amaphwanya malamulo ake . Vuto limeneli limapangitsanso kuti boma likweze misonkho kuti lipeze ndalama zimene zataika cifukwa ca ziphuphu . Pakali pano , atumiki a Mulungu ayenela kuyembekezelabe moyo wosatha . Magazini ya The Watch Tower ya September 1915 , inasintha kamvedwe ka mfundo imeneyo , ndipo inafotokoza kuti Ophunzila Baibulo ayenela kupewelatu kuloŵa usilikali . Naonso acinyamata angasinkhesinkhe pa zimene Yehova wawapatsa ndi kuwaphunzitsa . 26 Anamasuka Kucoka ku Cipembedzo Conama Kukhala munthu wauzimu n’kofunika ngako . Popeza sindinali kuopa aliyense , ndinali kutumidwa kukatenga ndalama zakaloŵa . Ndipo mofanana ndi Davide , tiyenelanso kupempha Yehova kuti atithandize kum’dziŵa bwino . N’zoziŵikilatu kuti io anganene kuti sangatelo . Ngakhale mavuto aang’ono , angaoneke aakulu ngati timangokhalila kuwaganizila . Aamoni anagonjetsedwa , ndipo amene anatuluka m’nyumba ya Yefita kudzam’cingamila pocokela kunkhondo atapambana , anali mwana wake wokondedwa . M’malo mwake iye anakamba kuti Mulungu ndi Atate wake . Pemphani Yehova kuti akuthandizeni kudziŵa zocitika zimene zingapangitse kuti cikhale covuta kupewa zandale . Mwacitsanzo , akulu angadziŵitse makolowo za thandizo limene boma limapeleka kwa okalamba . Zinali kugwilitsidwa nchito cabe pa kulambila koona . ( Eks . 4 : 17 ) Ndi umboni umenewu , Mose anali ndi cidalilo cakuti angapite kukakamba ndi Farao ndiponso ndi anthu a Mulungu . — Eks . Kodi Akristu angaphunzitse bwanji maganizo ao ndi cikumbumtima cao kuti apewe tsankho ? Pa cifukwa cimeneci , io amalephela kutsogolela bwino ana ao . Izi zimapangitsa banja kukhala losasangalala ndiponso losagwilizana . Mtumwi Paulo anacenjeza Agalatiya za kuopsa kolola anthu ena kuwapangila zosankha . Nkhani yopezeka pa lemba la Salimo 45 ndi yocititsa cidwi ndipo mapeto ake ndi osangalatsa . Lemba limene limanilimbikitsa ngako ni Yesaya 30 : 18 . Kodi Akristu amaona bwanji zimene Malemba amanena ponena za ciyembekezo cao ? Dzifunseni kuti : ‘ Ni mfundo za ndani zimene n’natsatila panthawi imene n’nasiyana maganizo na Mkhristu mnzanga ? Nimaona kuti nili m’banja la padziko lonse la abale okhulupilika , mmene muli mtendele weni - weni na mgwilizano . Kodi zinthu zimene timacita nthawi zonse potumikila Yehova , monga phunzilo laumwini , misonkhano , ndi ulaliki , zingathandize bwanji acinyamata ? Inde , pamene mau awa analembedwa , kulemekeza okalamba mumpingo kunali nkhani yofunika kwambili , ndipo n’cimodzi - modzinso masiku ano . Ndipo imanenanso kuti , “ akazi onse aluso amene anali ndi mtima wofunitsitsa anawomba nsalu za ubweya wa mbuzi . ” Iwo sadzasankha kutumikila Mulungu cabe cifukwa cakuti inu mumam’tumikila . Kapena mumaganiza za mwamuna wacikulile , wandevu zazitali , atavala mkanjo ndipo waimilila pamseu kwinaku atanyamula cikwangwani ca kutha kwa dziko ? ( Yohane 8 : 44 ) Motelo , tiyeni tikhale ocenjela ndi osamala kwambili ndi nkhani zambili zimene timalandila ndi kuona tsiku lililonse . Tatyana tsopano akutumikila monga mmishonale ku Russia . ( Mateyu 10 : 8 ) Atumiki onse amene amagwila nchito pa maofesi a nthambi ndi ku likulu lathu , komanso amene ali mu Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova , salandila ndalama . 6 : 6 , 8 ) Koposa zonse , tingaonetse kuti ndife odzicepetsa mwa kukhala omvela . Kodi Olaf anathetsa bwanji cizoloŵezi cokoka fodya ? Onani zinanso zimene Yehova wacitila anthu ake . ( 1 Yohane 4 : 7 , 20 , 21 ) Cifukwa cina n’cakuti timafunika kuthandizana , makamaka panthawi ya mavuto . Mlongo Ute wa ku Germany , wa zaka za m’ma 50 , anatumizidwa kukatumikila monga mmishonale ku Madagascar mu 1993 . Kodi ndingathe kum’fotokozela cifukwa cake ndimakonda masewela ena ake a pakompyuta ? ’ Mbusayo anauza mtsikanayo kuti : “ Milomo yako imangokhalila kukha uchi wapacisa . ” Zimenezi zimafuna kudzifufuza mosamala kwambili makamaka ngati munakulila m’coonadi . Kuonjezela pamenepo , tisataye mtima ngati taona kuti nchito yathu siikubeleka zipatso mwamsanga . Mai wina wa ku Ireland , dzina lake Christina , amene anali kupita ku chalichi mlungu uliwonse anati : “ Ndinali kuona Mulungu ngati amene analenga zinthu zonse cabe . Nanga bwanji ngati zimenezo sizidzacitika posacedwapa ? Kodi na imwe mumamvela monga mmene Sylviana anamvelela ? Mafanizo amenewa anam’thandiza kudziŵa ngati omvela ake anali ofunitsitsa kuphunzila ndi kutumikila Yehova . 144 : 15 ) Yehova ni Mulungu wacimwemwe , ndipo anthu ake amakhalanso acimwemwe . Kuyambila kale nsomba yakhala cakudya cofunika kwambili . Tikayamba kulakalaka zinthu zoipa , iye amaticenjeza kupyolela m’Mau ake , Baibulo . Yehova payekha ni wacikwane - kwane . Komabe , iye amakondwela akaona kuti tikuyesetsa kucilikiza ulamulilo wake . Anali kutanthauza gulu la asilikali amene anali kutumidwa kuti akateteze mzinda wokhala na mpanda wolimba kwambili . Ndiponso cionetsa mfundo yofunika yakuti : Sitiyenela kucita mantha kukambitsilana ndi anthu nkhani zovuta monga za Utatu , moto wa helo kapena nkhani ya kukhalapo kwa Mlengi . Pokambilana uthenga wa m’Baibo na munthu , tinali kuseŵenzetsa magilamafoni . 3 : 15 ) Mwacitsanzo , kodi ana anu angakwanitse kuseŵenzetsa Baibo pofotokoza zimene zimacitika munthu akamwalila ? Mwacitsanzo , Yesu ananena kuti : “ Inu munamva kuti anati , ‘ Usacite cigololo . ’ Anthu anali kumudziŵa kuti ndi mphunzitsi . 32 MLONGOZA NKHANI WA NSANJA YA MLONDA 2016 ( Deuteronomo 19 : 15 ) Motelo iye analemba makalata m’dzina la Ahabu , ndi kulamula anthu olemekezeka a ku Yezereeli kuti apeze anthu aŵili amene angalole kupeleka umboni wonama wotsutsana ndi Naboti . ( 1 Tim . 4 : 15 , 16 ; 1 Pet . Nthawi zina kukhala wokhulupilika kwa Yehova kumakhala kovuta . Komabe , Ufumu wa Roma unakhala wamphamvu kwambili ndi waulemelelo cifukwa cogwilitsila nchito akapolo . Ife Mboni za Yehova , sikuti timangoyelekezela mwaciphamaso kuti ndife abale ndi alongo . Anadziŵa kuti Yehova ndi Mtetezi wacikondi ndi Wosunga malonjezo . Ngakhale m’nthawi ya atumwi , Paulo analangiza Akristu anzake kuti apewe ‘ kaganizidwe kamene kakugwila nchito mwa ana akusamvela ’ kamene io “ panthawi inayake ” anali kuyendamo . Tikafika pa cisumbu , anthu a kumidzi imeneyo anali kucita cidwi , ndipo anali kufika pafupi kuti adziŵe kuti ndife ndani . Cifukwa ca kusamvela kwa Aisiraeli , Yehova analeka kuwateteza kwa adani ao . Kodi tate wina anacita ciani kuti asamalile banja lake ? Nanga Yehova anadalitsa bwanji cosankha cake cokhala ndi umoyo wosalila zambili ? Tikamaganizila zofooka za Akristu anzathu , tingayambe kuona zofooka zao moyenelela . Debora anadziŵa kuti Baraki ndi gulu lake lankhondo akuyembekezela mau kapena cizindikilo kucokela kwa iye . Zoonadi , Mulunguyo adzakhala nao . N’ciani cinapangitsa Lefèvre kumasulila Baibo m’Cifulenchi ? Anaŵauza kuti iye anali wovutika maganizo kwambili . Conco , iwo anam’limbikitsa mwa kukambilana naye malemba otonthoza a m’Baibo . Komabe , colinga ca utumiki wake sicinali cofuna kulimbikitsa anthu kusintha zinthu pa zandale ndi pa zacikhalidwe , olo kuti zimenezo n’zimene ambili pa nthawiyo anali kulakalaka . “ Sitinabwele ndi kanthu m’dziko , ndipo sitingatulukemo ndi kanthu . Komanso tingakhale ndi cidalilo cakuti Baibulo lidzatithandiza kupitilizabe kusintha umunthu wathu . — Salimo 34 : 8 . Ngakhale kuti nthawi zina kulankhula mau amenewa kungakhale komveka , Baibulo limanena kuti : “ Usanene kuti : ‘ Ndim’citila zimene iye anandicitila . ’ ” Yehova amaona kuti misonkhano yathu ndi yofunika kwambili moti anauzila mtumwi Paulo kulemba mau otilimbikitsa kuti tisaleke kusonkhana pamodzi . 3 : 12 - 14 . ( b ) Tidzakambilana ciani m’nkhani yotsatila ? Nthawi zambili , iye anali kupempha Mulungu kuti amutsogolele . N’ZOONEKELATU kuti Adamu anali kudziŵa kuti njoka siingakambe . Pambuyo pakuti waŵelenga kabuku kameneko , John anazindikila kuti zimene anali kuŵelengazo ni coonadi ca m’Baibo . Awo amene ali ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi adzachedwa ana a Mulungu enieni , akadzakhala angwilo ndi kupyola ciyeso comaliza . — Aroma 8 : 21 ; Chiv . Kodi mkazi wacikhristu angakope bwanji mwamuna wake amene si Mboni kuti ayambe kulambila koona ? ( Mat . 24 : 10 - 12 ) Ngakhale kuti anthu kulikonse anali kudzamvetsela uthenga wao , kodi io akanakwanitsa bwanji kulalikila “ mpaka kumalekezelo a dziko lapansi ” ? ( Mac . Koma patapita zaka 40 , vuto lofanana ndi limeneli linabukanso pakati pa Aisiraeli , cakumapeto kwa ulendo wawo wa m’cipululu . Ndipo ndi nzelu kusankha kucita zimenezi m’malo mongotsatila acinyamata ena mopanda nzelu ndi kuonongedwa limodzi ndi dzikoli . — 2 Akor . Pamenepa , Yesu anaonetsa kuti munthu aliyense amene wasankha kukhala wotsatila wake , afunika kubatizika . ( Mat . Inu Mulungu wanga , ine ndataya mtima . Ndine m’bale wanu . ” 112 : 5 ; Miy . Nanga a “ nkhosa zina ” angaike motani maganizo ao pa “ zinthu zakumwamba ” ? ( Onani bokosi lakuti “ Mmene Tingaphunzitsile Ena . ” ) Mungatengele bwanji citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wacifundo ? N’zoona kuti ndise “ abale ” cifukwa tonse tinabadwa kucokela kwa Adamu . Mosiyana ndi akatswili a zacipembedzo a m’nthawi yake , iye anayesetsa kupeza njila yofotokozela mavesi a m’Baibo “ momveka bwino . ” Citsanzo cake cinaniphunzitsa kuti ngati munthu wadzicepetsa pa maso pa Mulungu mwa kulandila cilango cake , amalandila madalitso oculuka . ” Kodi Baibulo limapeleka malangizo otani kwa atumiki a Yehova amene ali pa banja ndi wosakhulupilila ? Baibulo limati : “ Kunena za tsikulo kapena ola lake , palibe amene akudziŵa , ngakhale angelo kumwamba kapenanso Mwana , koma Atate okha . Nthawi ina , iye anapezeka pa “ phwando la ukwati ” komanso pa phwando lina lalikulu . Iye anadziŵa kuti anakhala na maluso , mphamvu , na maudindo cifukwa cakuti Mulungu ‘ anatsika m’munsi , ’ kapena kuti anadzicepetsa , kuti amuthandize . ( Sal . Ofatsa ni anthu amene amamvela modzicepetsa malangizo a Yehova ndi ziphunzitso zake . Olungama ni anthu amene amakonda kucita zoyenela pamaso pa Yehova Mulungu . ( b ) Ndi madalitso ati amene tidzapeza ngati tikumbukila Yehova m’njila zathu zonse ? Mulungu amaona zolakwa moyenela . PACIKUTO : Mboni za Yehova zimagwilitsila nchito maboti kuti zikalalikile anthu amene amakhala ku zilumba za Bocas del Toro ndi Archipelago kumpoto cakumadzulo kwa dziko la Panama . 15 : 28 , 29 ) Timacita mantha tikaganiza zocita zinthu zimene zingacititse kuti Mulungu atikane ndi kuticotsa mumpingo wake . Mungamuthandize kukonzekela misonkhano kuti akayankhepo . 27 : 1 , 14 ; Mac . 24 : 15 ) Koma kuti ‘ cisote ’ cathu cimeneci cititeteze bwino , tifunika kucivala osati kucinyamula kumanja . Kodi Yehova amakugwilitsilani nchito kuti muthandize ena kuti ayambe kumuona ? 7 : 13 ) Yesu sanaope kapena kunamizidwa , koma anacitila cifundo anthuwo ngakhale kuti sanakumanepo ndi vutolo . Mungathandize bwanji atumiki anthawi zonse amene akutumikila m’dziko lanu ? Nkhani yake ndi yakuti mtsikanayo anali kugwila nchito m’munda wa mpesa wa mlongosi wake . Kodi tidzapewelatu kunama na cinyengo ciliconse ? Mwacionekele , Davide anaphunzila kugwilitsila nchito cida cimeneci pamene anali m’busa wacicepele . — 1 Samueli 17 : 40 - 50 . Kulemba Baibulo kunatenga zaka zoposa 1,600 . Iye anati : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” ( Mat . Mwina bungwe lina lake la boma lingakuuzeni nchito zimene n’zofunika kwanuko kapena ku dela limene mufuna kukatumikila . Muzipempha mzimu woyela , nzelu zake ndi citsogozo cake . Mu 1991 , nchito ya Mboni za Yehova inakhazikitsidwa mwalamulo . ( Mateyu 5 : 9 ) Yesu anacita zimene anali kuphunzitsa mwa kupewa ciwawa ndi kulalikila uthenga wa mtendele kwa anthu a zipembedzo zosiyana - siyana . 19 : 2 - 4 . Ngakhale kuti sitingakonde njila zimene anagwilitsila nchito , palibe amene angasulize colinga cao . Kumeneko , apainiya apadela anali kulalikila m’magawo amene kunalibe Mboni . Kutatsala masiku ocepa kuti ayende m’munda wa Getsemane , Yesu anauza ophunzila ake amodzi - modziwo kuti alimbikile kupemphela kwa Yehova . Kodi mungakonde kupeleka kapena kulandila mphatso yabwino kwambili ? 4 : 4 ) Conco tiyenela kupemphelabe kuti Yehova apitilize kutipatsa cakudya ca kuuzimu panthawi yake . M’caka ca 1941 , n’nayamba umoyo umene wanithandiza kukhala wacimwemwe . Iye anasankha anthu ena odzipeleka kuti akhale “ ana ” mwa kuwadzoza ndi mzimu woyela . Conco ndi mwai wamtengo wapatali kukhala pakati pa anthu amene Yehova wawakokela kwa iye mokoma mtima , ndi kuwavumbulila coonadi ca m’Baibulo . 3 : 16 ; Chiv . Ndithudi , mbeu ya Davide “ idzakhala mpaka kalekale , ndipo mpando wake wacifumu udzakhala ngati dzuŵa . ” ( Sal . Kodi akulu angatengele bwanji cilungamo ca Mulungu poweluza mlandu wa munthu amene wacita chimo ? Maluso athu mwa iwo okha si kanthu . Kukhala na nkhawa komanso kusoŵa tulo Ndipo anali kucidya limodzi ndi mkate wocedwa pita . Onse anali kudzinenela kuti anali kulambila Yehova , koma sanali okhulupilika kwa iye . ( Aroma 8 : 22 ) N’ciani cinacitika ? Iye anati : “ Nchitoyi ikukula kwambili ndipo idzapitiliza kukula cifukwa cakuti ‘ uthenga wa Ufumu ’ uyenela kulalikidwa padziko lonse . ” Yehova ndi wacikondi cacikulu ndi wacifundo . ( Mungawatenge kuti muyendeyendeko nao , museŵeleko nao , kapena mugwileko nao nchito za panyumba . M’malomwake , anamvela uphungu wocokela kwa anyamata anzake amene anakula nawo , amenenso panthawiyo anali atumiki ake . “ Mau a Mulungu . . . Baibulo limakamba momveka bwino kuti sitiyenela kuloŵa m’banja ndi munthu amene satumikila Yehova . Conco dzifunseni kuti , ‘ Kodi colinga canga coonjezela utumiki ndi kufuna kuchuka kapena kukhala ndi udindo , monga mmene zinalili ndi Yakobo ndi Yohane pamene anapempha Yesu kuti akakhale pamalo apamwamba ? ’ Zofalitsa zosiyanasiyana zimenezo zimaonetsa kuti Yehova akukwanilitsa lonjezo lake lakuti adzapeleka malangizo ambili kwa anthu onse . — Yesaya 25 : 6 . Ndipo ngati tigonjela kuulamulilo wake ndi kumumvela , tidzakhala ndi moyo wamtendele ndiponso wopindulitsa . Cifukwa coyamba cimene timakhulupilila kuti Yesu anaukitsidwa n’cakuti kuuka kwake kunacitika “ malinga ndi Malemba . ” Mitengo ina mukaiwoka , imatenga nthawi itali kuti igwile kusiyana na ina . Ndimasinkhasinkha cilamuloco tsiku lonse . ” — Sal . Mau amene ali pamwalawo sakuonekela bwinobwino , koma ayenela kuti anali kunena kuti : “ Tiberieum ( iyi ) nyumba imene Pontiyo Pilato , Bwanamkubwa wa ku Yudeya , anapeleka kwa milungu yolemekezeka . ” ( Mat . 28 : 19 ) Makhalidwe amenewa amatithandizanso kuti tizikhala bwino ndi abale na alongo athu onse mumpingo . Kuganizila zinthu zabwino Kukambilana ndi anthu momasuka . MAPINDU AMENE NDAPEZA : Pamene ndinali ndi mzimu wodzikonda , sindinali kukhala wotsimikiza popanga zosankha . 5 : 13 - 15 ) Musacedwe kucita zimenezi , cifukwa tsogolo lanu lili paciwopsezo . 34 : 4 , 15 , 17 ; Dan . 9 : 19 - 21 ) Ifenso tingamuuze Yehova nkhawa zathu podziŵa kuti iye adzatimvela ndi kutilimbikitsa kuti tipilile mosangalala . Conco , tiyeni titsimikize mtima kutengela citsanzo ca Yesu . Thonje limayamwa zilizonse zamadzi zimene mwaliikamo . Kodi mwamuna wacikhristu angaonetse bwanji kuti amakonda mkazi wake ? “ Imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . ” — Chivumbulutso 21 : 4 . N’cifukwa ciani n’nasankhidwa ? 14 : 20 . Muziona thandizo lawo monga umboni wa cikondi ca Mulungu pa imwe . Cifukwa ca lonjezo limenelo , mtsikanayo sakanakhala ndi mwai wokwatiwa kapena kukhala ndi ana . Mkupita kwa nthawi , n’nabwelelanso ku Saskatoon . ( Salimo 90 : 14 ) Ndife odalitsidwa cifukwa timakwanitsa kuona ndi kukhulupilila cikondi ca Yehova pa ife . M’nkhani ino sitingakambe za mavuto onse , koma tidzakambilana za mavuto anayi amene tawachula poyamba paja . Mwacitsanzo , Yehova anauza Ayuda kuti : “ Mzinda umene ndakucititsani kukhalamo monga akapolo , muziufunila mtendele . ” ( Yer . Conco , zioneka kuti cimene anthu anali kunyamula kweni - kweni ni zoyatsila moto . Ni zinthu zabwino ziti zimene mungaphunzile ngati mugwila nchito yopanga ophunzila ? 3 : 1 ) Nthawi zonse , iwo afunika kuonetsetsa kuti zimene amaphunzitsa n’zozikidwadi m’Mau a Mulungu . 3 : 2 - 5 Ndipo zina mbali yaikulu kulibe . Sindinali kufuna kuti Akristu anzanga aziona kuti ndine munthu wabwino pamene sindinali conco . ” * Iye sanali kukonda ulaliki ngakhale kuti anali kulalikila kaŵilikaŵili . Magazini ino ya Galamuka ! Tikukhala m’dziko lodzaza ndi upandu , ndipo eninyumba amacita mantha kucezeledwa ndi anthu acilendo . ( 2 Tim . M’kupita kwa nthawi , mantha anayamba kutha ndipo n’nakhala na cidalilo . Atacita izi , mwanayo anauka ndipo anam’peleka kwa amayi ake . Iwo anakondwela ngako ! ( Luka 6 : 35 ) Yehova waonetsa cifundo cake mwa kukhala woleza mtima . Kucokela panthawiyo , Akristu onse akhala akutsatila Cilamulo cimeneci , ndipo akupindula . — Agalatiya 6 : 2 . N’ciani cingaticititse kuwononga ubwenzi wathu na Yehova ? Koma mngeloyo sanafotokozele banja la Mariya ndi anzake za mmene Mariya adzakhalila ndi pakati . Kodi inu panokha mumaona dzanja la Yehova pa umoyo wanu ? Kodi mumapindula mokwanila pamene muphunzila Baibulo ? Kuika zofuna za ena patsogolo mwanjila imeneyi , kumaonetsa kuti ali na cikondi copanda dyela . M’malo moyamikila kubwela kwa Mesiya , amene ndi mbali yoyamba ya mbeu ya Abulahamu , Aisiraeli anamukana . Koma panthawiyo Akristu onse oona adzakhala ndi mwai woonetsa kuti amakondadi Yehova ndi kucilikiza abale a Kristu . — Mat . 15 : 33 . Ponena za makhalidwe oipa , iye anawauza kuti : ‘ Muwataye kutali ndi inu . ’ 9 : 11 , 12 . Mdyelekezi anauza Hava kuti ngakhale ataphwanya malamulo a Mulungu , sadzafa , ndipo ananena kuti Mulungu ndi wabodza . Nthawi zina ndalama zimene ndinali kupeza zinali zocepa kugulila zofunikila , ndipo ndinali kukhala wotopa . Tinali kuona kuti zinali zosangalatsa olo kuti zinali zocititsa mantha . Ndipo si bwino kumangoganizila zolakwa zawo . UKAKUMANE NDI AHABU ” Mfundo yaikulu ni yakuti , sitiyenela kumangoganizila zocitika za pa umoyo wathu mpaka kufika poiŵala nkhani yofunika kwambili , imene ndi kucilikiza ulamulilo wa Yehova . Komabe , anthu mamiliyoni ambili apeza cinthu camtengo wapatali kuposa golide . Nkhani ino yafotokoza cinthu cimodzi cimene cingakuthandizeni kukhala acimwemwe . Pa www.jw.org / nya Conco ndi cinthu canzelu kupitilizabe “ kufunafuna ufumu coyamba ” ndi kuika maganizo athu pa madalitso amene timalandila cifukwa cotumikila Yehova . — Mat . ( 1 Akorinto 16 : 2 ) Mwezi uliwonse mipingo imatumiza zopeleka zimenezi ku ofesi ya Mboni za Yehova m’dziko lao . Kodi iwo anali kumvela bwanji m’zaka zimene anali kucita utumiki umenewo ? Buku lochedwa The World Book Encyclopedia limakamba kuti ufulu umatanthauza “ kukhala na mwayi wopanga zosankha na kuzikwanilitsa . ” Amenewa ndi angelo audindo wapamwamba kwambili . Amatiphunzitsanso kukhala ndi maganizo oyenela . Kodi inu mungayeseko kumvetsela Baibo pocita zina mwa zinthu tachulazi ? Ise sitili monga mkaidi amene ali m’ndende woyembekezela kunyongedwa . Mu mtima , wacicepele angakambe kuti , ‘ Yehova anakoka makolo anga , koma ine n’nawakonkha cabe . ’ Paciyambi , Satana mdyelekezi kupitila mwa njoka monga cobisalilamo , ananamiza Hava , mkazi woyamba ndipo anadzionetsa ngati wabwino pofuna kum’soceletsa . Kutenga anthu ukapolo mu Africa na kupita nawo ku America anali malonda opindulitsa Silikamba kutalika kwa mtunda umene unalipo kucokela kumene Yesu analili kufika ku Yerusalemu , kapena utali wa nthawi imene iye anayesedwa ndi Satana . 9 : 19 - 23 . ( Machitidwe 2 : 34 ) Yehova anapatsa atumiki ake amenewa mzimu woyela kuti acite zinthu zazikulu . Koma sanawadzoze ndi mzimuwo kuti adzapite kumwamba . Tifunika kuiŵelenga , kuganizila mozama pa zimene taŵelenga , ndi kupempha Yehova kuti atithandize kugwilitsila nchito zimene taphunzila . Onani kuti Ribeiro sanangoŵelenga Baibo cabe kuti aleke cizoloŵezi cotamba zamalisece . Yehova wathandiza amuna ambili kupezanso cimwemwe ndi kukhala ofunitsitsa kutsogolela mu mpingo . Pamene tiitanila ophunzila Baibulo ndi anthu ena ku mwambo wa Mgonelo wa Ambuye , timasangalala kuuza ena za Mulungu , Mwana wake , ndiponso za madalitso amene Yehova wasungila anthu amene amam’tamanda ndi kucita zinthu zomukondweletsa . — Sal . Maguluwo anayenda kuloŵela mbali ziŵili zosiyana , ndipo anakumana pafupi na kacisi . Oimbawo anali kuimba mokweza kwambili cakuti mau awo anamveka kutali . ( Neh . ( 2 Mbiri 16 : 5 ) Conco , zimene Asa anacita , zinaoneka monga zathandiza . Cilamulo ca Mulungu kwa Aisiraeli cinali kusonyeza kuti oweluza afunika kukhala ndi makhalidwe amenewa . Kodi kudzicepetsa kungatithandize bwanji kupanga zosankha zabwino ? Phunzilo laumwini na kusinkha - sinkha n’zinthu zofunika kwambili zimene zingatithandize kukonza cipulumutso cathu . — Ŵelengani Salimo 119 : 105 . Yehova afunanso kuti tizim’konda ndi ‘ maganizo athu onse ’ komanso ‘ mphamvu zathu zonse . ’ Atate wathu wakumwamba sadzakutayani nonsenu abale ndi alongo athu okalamba . Sitidzakhala na nkhawa kwambili kapena kudziimba mlandu . ( a ) Pambuyo poukitsidwa , kodi Yesu anapeleka lamulo lanji kwa otsatila ake ? Iye anafelanso onse kuti amene ali moyo asakhale moyo wongodzisangalatsa okha , koma akhale moyo wosangalatsa amene anawafela n’kuukitsidwa . ” Padziko lapansi pali anthu mabiliyoni ambili . Masiku ano tili na umboni woculuka woonetsa kuti tili m’nthawi imene Baibo imacha kuti “ masiku otsiliza . ” Ena mwa iwo ndi aserafi ndi akerubi . Cifukwa cakuti anali kufunitsitsa kucila , iye anayankha mwamsanga , koma anali ndi nkhawa kuti adzacila bwanji popeza kunalibe womuviika m’dziwe . Tikukhala m’nthawi yapadela . M’nyumbayi mulinso Mabaibo amene sapezeka - pezeka masiku ano , ndi zinthu zina zakale zocititsa cidwi zokhudzana ndi Baibo , zimene zidzayamba kusinthidwa - sinthidwa m’kupita kwa nthawi . Mosiyana ndi Aisiraeli osayamika a m’nthawi ya Mose , tingaonetse bwanji kuti timayamikila mkate umenewo wamtengo wapatali ? Koma abale ndi alongo mumpingo akamacita zilizonse zotheka kuti Nyumba ya Ufumu izioneka bwino , Yehova amatamandidwa ndiponso zimathandiza kuti ndalama zimene abale amapeleka zisaonongeke . Koma anthu a Yehova amafuna kuti cikumbumtima cao cizigwila bwino nchito cifukwa cingawathandize kukhala pamtendele ndi ena mumpingo . Nanga n’ciani cina cimene cinali colingana pa anthu aŵiliwa ? 5 : 3 ) Kucita zinthu za kuuzimu ndi cinthu cacikulu cimene tizidzacita m’dziko latsopano ndipo tidzaonetsa kuti tikusangalala kwambili mwa Yehova . N’kuthekanso kuti makolo ena mumpingo amalola ana awo kucita zinthu zina zimene imwe simufuna kuti ana anu azicita . Kodi cikondi ca Mulungu cidzakhudza bwanji tsogolo la anthu amene amamumvela ? Satana amaseŵenzetsa njila zamacenjela pofuna kusoceletsa anthu . Timayamikila tikaona acinyamata amene amatumikila abale ndi alongo modzipeleka . — Ŵelengani Salimo 110 : 3 ; Mlaliki 12 : 1 . Kumathandiza munthu kukhala pa ubwenzi wabwino na ena , kuphatikizapo kukomela mtima munthu amene wamulakwila , kumumvesetsa , na kum’citila cifundo Cioneka kuti lomba nakalamba . Fanizo la matalente ndi la mina ndi ofanana m’njila zingapo . Kodi Akristu ena acita ciani kuti ayambe kutumikila Mulungu m’njila zina pamene akukalamba ? Yehova amafuna kuti imwe mukhale bwenzi lake . 103 : 10 ) Koma Yehova anaona zabwino mwa ife . Ganizilani izi : M’citsanzo ca munthu amene “ amadziyang’ana ” pagalasi , Yakobo anagwilitsila nchito liu lacigiliki limene limatanthauza kudzifufuza mosamalitsa . Ŵelengani Luka 4 : 43 . Ambili mwa iwo anasiya zonse zimene anali kucita kuti akatumikile kumeneko . Kukhala bwino ndi anthu ena Nayenso Andre , amene ali ndi zaka 23 , anakamba zofanana ndi zimenezi . Malinga ni luso lawo , ngakhale ana aang’ono kwambili angathe kumvetsa zinthu zosavuta monga zokhudza anthu na zocitika za m’Baibo . Nkhaniyi idzayankha mafunso amenewa . Amy anakamba kuti kupanga ubwenzi ndi mlongo wofikapo wa ku maloko kunamuthandiza kudziŵa zikhalidwe zosiyanasiyana za kumeneko . Mfundoyi imakhudza mmene mwininyumba amadziŵila Baibulo . Colinga cawo cinali cogwilizana kwambili na cifunilo ca Mulungu cakuti “ anthu , kaya akhale a mtundu wotani , apulumuke ndi kukhala odziwa coonadi molondola . ” — 1 Tim . Kenako mu 2005 , linapeleka cilolezo cakuti omasulila amene amamasulila Nsanja ya Mlonda m’zinenelo zao , amasulilenso Baibulo m’zinenelo zimenezo . Tiyenela kuonetsa cikondi cimeneci kwa onse , osati kwa anthu a mtundu wathu cabe . Ufulu umene mzimu wa Yehova umabweletsa , ni wapamwamba ngako kuposa ufulu umene munthu amakhala nawo akamasulidwa mu ukapolo wakuthupi . Nthawi zambili amapita kumzinda kukagulitsa zinthu zokongola zimene amapanga . Kale , anthu anali kupita ku Isiraeli kukatumikila Yehova . Pempho limeneli lingakusonkhezeleni kupempha Yehova kuti akuthandizeni kupewa kucita kapena kukamba zinthu zilizonse zosalemekeza dzina lake lopatulika . Yesu anati : “ Odala ndi anthu amene amazindikila zosoŵa zao zauzimu , cifukwa ufumu wakumwamba ndi wao . ” ( Mat . NTHAWI : Muzisankha nthawi yabwino yokamba zinthu 7 : 29 - 31 ) Paulo sanatanthauze kuti Akhiristu azinyalanyaza maudindo awo a m’banja ayi . Yehova Mulungu na Yesu Khiristu ni zitsanzo zabwino ngako pankhani yolimbikitsa ena . Yehova anacita zonsezi cifukwa cotikonda , osati kuti apindulepo kenakake . NYIMBO : 125 , 88 Anadzipeleka na Mtima Wonse ( alongo osakwatiwa ) , Jan . Tidzasangalala ndi moyo m’paradaiso weniweni pamene Ufumu wa Mulungu udzayamba kulamulila dziko lonse . Koma cifukwa ca ucimo umene tinatengela kwa makolo athu , cimakhala covuta kwa ise kuonetsa cikondi . Mwamuna wina wa banja lacatsopano , anakamba kuti khadi yokondwelela caka coyamba ca cikwati cawo imene mkazi wake anamukonzela inali mphatso yoposa zonse zimene analandilapo . Angelo ni “ amphamvu ” kwambili kuposa anthu , ndipo ali na nzelu zakuya kutipambana . Simone anati : “ Anthu m’gawo lathu ni aubwenzi komanso ambili ni acidwi . M’malo moweluzilatu kuti m’baleyo sayenela kukhala mkulu , kodi mudzayembekezela moleza mtima kuti Yesu , mutu wa mpingo , adzacitapo kanthu ? M’malo mwake , kuyenela kuticititsa kukhala paubwenzi wolimba ndi Mulungu amene amatisamalila kwambili . [ Mau apansi ] Ni buku yolinganizika bwino , youzilidwa na Mulungu . Conco , mwina n’kutheka kuti pamene Mose anamenya thanthwe lofookalo kaŵili , anthu anaganiza kuti iye wangobooleza madzi m’thanthwelo , osati kuti Yehova ndiye watulutsa madziwo . Pamene Yosefe anafika ku Dotana , abale ake anamuonela patali . Kodi Munakhumudwa ndi Mulungu ? Gumbwa ndi zomela zinazake za m’madzi zimene kale anali kupangila mapepala . Ndipo ife abale a ku nthambi tinali kuwakonda kwambili abalewo , cifukwa anatumikila movutikila zaka zambili pamene nchito inali yoletsedwa . Sara anakwatiwa ndi Abulahamu , amene anali kum’posa na zaka 10 . Conco , ndife oyamikila kwambili kuti Yehova analemba Baibulo mwa njila yosavuta kuimvetsetsa . Patapita miyezi 9 , Mboni yacikondi ndi yokoma mtima imeneyi inayamba kundiphunzitsa Baibulo moleza mtima . Malinga ndi zimene wolemba mbili wina wochedwa Eusebius ananena , anthu ambili anadutsa Mtsinje wa Yorodani ndi kuthaŵila ku Pela mumzinda wa Pereya . ( Ŵelengani Aroma 14 : 12 . ) Komabe , wodulila maluŵa amafunika kusamala podula , cifukwa ngati sanatelo maluŵa angafote kapena kuuma . Kodi nkhani ya pa Oweruza 6 : 11 - 16 , ionetsa bwanji kuti Yehova amaona zimene atumiki ake angathe kucita ? Fotokozani zitsanzo za mmene Yehova waonetsela kuti amawayanja anthu ake . Koma atumiki a Yehova ndi osiyanako . Nakwanilitsa colinga canga . ’ ” — Christopher . Ndi zabwino komanso zosangalatsa kwambili . . . kukhala pamodzi mogwilizana ! ’ — SAL . Iye anam’pepesa Janet , ndipo lomba iwo atumikila Yehova mogwilizana . N’cifukwa ciani tidzakambilana ena mwa maganizo amene anthu ali nawo m’dzikoli ? Nkhaniyi ionetsa kuti banja la Abulahamu linali kupanga lokha mkate . Komabe , nthawi zina pamakhala acicepele ena amene amaoneka kuti alibe mayankho . Atacoka ku msonkhano , mkaziyo anaona kuti si canzelu kupita ku cikondwelelo cimene cingaike moyo wake wauzimu paciswe . Mmodzi wa olemba nkhani zokhudza Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa anakamba kuti mpukutu umodzi “ ndi wokwanila kupeleka umboni woonekelatu wakuti anthu Aciyuda amene anakopela mawu a m’Baibulo pa zaka zopitilila 1000 anali okhulupilika ndi osamala kwambili . ” Ndipo amaonetsa cikondi cimeneci mwa kucita cifunilo ca Yehova osati cake . Koma ngati tipatsa ena uphungu , kapena kuwaongolela sizitanthauza kuti tilibe cikondi . Panthawiyo n’nali n’tayamba kuphunzila nchito yokonza maboti pa kampani ina yochedwa Royal Dockyard mu mumzinda wa Chatham . Zaka 20 m’mbuyomo , M’bale Russell anaganiza zoyamba kuyenda m’maiko osiyana - siyana a kunja kwa dziko la America , pofuna kupeza njila yabwino yofalitsila uthenga wabwino padziko lonse . ( Ŵelengani Mateyu 9 : 37 . ) ( Sal . 141 : 3 ) Kumbukilani kuti ngati munthu acita zinthu ali wokwiya , n’zosavuta kulakwitsa . Kodi mlongo wacikulileyo anamvela bwanji atakukila ku dziko lina ? A Daka : Sindinaganizepo conco . Koma zimene mwanena n’zoona . 11 : 42 ) Solomo anamwalila mu 997 B.C.E . Mwalawo unamenya Goliyati pamphumi ndi kuloŵelatu m’mutu mwake . Koma kuwonjezeleka kwa makhalidwe oipa na ciwawa kumatitsimikizila kuti mapeto a ulamulilo wawo woipa ali pafupi . 27 : 11 ) Anthu ambili m’dzikoli ali na maganizo olakwika pankhani yolemekeza ena . Motelo , akulu amene akutumikila m’madela osowa ali ndi nchito yofunika kwambili yothandiza abale a m’madelawo kukhala abusa a nkhosa . Itafunsidwa ngati inali kumvetsetsa zimene inali kuŵelenga , inayankha kuti : “ Ndingamvetse bwanji popanda wondimasulila ? ” Cifukwa ca ici , ndimaona kuti ndikuyenda ndi Yehova . ” Iye anati : “ Ndinali kulalikila maola ocepa cifukwa sindinali kusangalala ndi ulaliki . ” Kodi tidzamvela bwanji mavuto akadzatha ? Pambuyo pake , Zera Mwitiyopiya anabwela kudzamenyana ndi Ayuda ali ndi asilikali 1,000,000 ndi magaleta 300 . Iye anati , “ Ndimakondwela kuti tonse timakhala pamodzi ndi kukambilana . Mokondwa apainiya anaika maganizo awo pa ulaliki wakumunda Mphoto imeneyo si loto cabe . Koma cimfine ca ku Spain cinali ciyambi cabe . ( Sal . 119 : 5 , 6 ) Mtsogolo , Satana akadzaonongedwa , tidzakhala ndi moyo wosatha m’dziko latsopano lopanda makhalidwe oipa . Mumakhalanso na mphamvu yolimbana ndi zopinga za tsiku na tsiku . Mwacitsanzo , mumatha kukana kutunthiwa na anzanu . Kodi Akristu a m’nthawi ya atumwi anali kugwilitsila nchito ciani kuti aphunzitse Malemba mu utumiki ? Tikatelo , tidzaonetsa kuti timakonda ndi kucilikiza ulamulilo wake . 12 , 13 . ( a ) Kodi zimene Yosefe anakamba kwa wopelekela cikho , zinaonetsa bwanji kuti sanadzilekelele pa mavuto amene anakumana nawo ? Nditacita cidwi ndi zimene anali kuphunzila , inenso ndinayamba kuphunzila . 8 Makolo , Kodi Mukuthandiza Ana Anu Kupita Patsogolo Kuti Akabatizike ? Iye anadziŵa kuti chimo limene anacita ndi Batiseba ndi limene linabweletsa mavuto m’banja lake . Mwacitsanzo , Davide analemba kuti “ wokhulupilika ” wamkulu wa Mulungu sadzasiidwa m’Manda . Sindimvetsetsa kuti n’cifukwa ciani ndimacita zinthu motele . Lipoti la ulaliki loyambila mu 1928 mpaka mu 1937 imene inalembewa patsamba loyamba , inaonetsa kuti zimenezi n’zoonadi . Nthawi zina ungaone kuti mwana wako wamuyankha mom’khutilitsa pa funso lake . Apa Yesu anali kunena za imfa yake . ” — Yohane 11 : 11 - 13 . Ngati tivala mwaudongo , mwaukhondo , mwaulemu , ndi kudzikonza bwino , anthu adzatilemekeza monga atumiki a Yehova . Nimakumbukila funso locititsa cidwi limene ena anafunsa , lakuti : Ngati tauzidwa kuti tidzalandidwa zonse zimene tili nazo , kupatulapo zokhazo zimene tinamuyamikila Yehova dzulo , kodi imwe mungatsale na ciani ? ” N’cifukwa ciani mlongo wina ndi wotsimikiza kuti Yehova amadziŵa zimene tikufuna ? M’banja lathu , ndine mwana waciŵili pa ana 8 . Pamene n’nakwanitsa zaka 8 , ambuye anga ananitenga kuti nizikakhala nawo . Colinga canga cinali cakuti nionetse kuti zimene a Mboniwo anali kuphunzitsa n’zabodza . Yehosafati anafunika kukumbukila kuti maso a Yehova ali pa anthu amene mtima wawo uli wathunthu kwa iye . N’ciani cidzacitika akadzapempha thandizo panthawi imeneyo ? Ndithudi , Akristu a 144,000 amene ali m’gulu la mkwatibwi adzasangalala kwambili . Ndimapita kukagulitsa sopoyu ndi njinga yanga ya mawilo atatu . ( Ezara 1 : 1 - 4 ) Koma adani a Ayuda anafuna kulepheletsa nchito yomangayo , ndipo inakhala cifukwa cowapatsila mlandu wopandukila ufumu wa Perisiya . Koma anadalila Yehova . CIKUTO : Alongo aŵili alalikila kwa anthu amene akuyenda mumseu waukulu pafupi ndi mapili a Mbololo , kum’mawa koma cakum’mwela pang’ono m’tauni ya Tausa , ku Taita 20 : 26 , 27 ) Daniel anakamba kuti : “ N’namvela monga kuti Yehova akukamba na ine . ” Mwa ici , cikwati cinacokela kwa Mulungu . Mame ndi ofunika kwambili pa moyo . Taona bwino lomwe kuti Baibo ili na uphungu wothandiza pa kupewa mavuto aakulu . N’cifukwa ciani tiyenela kuona nkhani ya kulimbikitsana kukhala yofunika kwambili masiku ano ? Zimene banjalo linakamba zinali ngati akuuza Choong Keon ndi mkazi wake Julie . ( Yakobo 1 : 13 ) Mulungu sayesa munthu aliyense mwa kum’cititsa kukhala ndi khalidwe loipa . 6 : 2 , 3 ) Kucita zinthu mwa njila imeneyi kudzam’fika pamtima mwana wanu . Anali kufunika kuthaŵila ku umodzi mwa mizinda yothaŵilako imene Yehova anakhazikitsa . Ngati sanatelo , m’bululu wa wophedwayo anali kuloledwa kumupha . Pamenepa , tinaona kuti Yehova anatiteteza . Makolo anu ayenela kuti anayamba kukuphunzitsani muli wakhanda . 2 : 18 , 19 . ( 2 Mbiri 16 : 9 ) Ngakhale kuti Yehova anaona kuti Asa analibe mtima wathunthu , iye ‘ adzaonetsa mphamvu zake ’ kwa inu ngati mucitabe zinthu zabwino . Ponena za mnyamata wina dzina lake Julien , amene anali wamanyazi , Ludovic anati : “ Iye anali kuyesayesa kuti acite zambili mu mpingo koma anali kudzikaikila . Zitadzacitika conco , kodi tingadzaonetse kuleza mtima ndi kusangalala ndi anzathu ? Ndinali kudzifunsa kuti , ‘ N’cifukwa ciani Mulungu analenga anthu ? Nanga pali phindu lotani kuti munthu amene akuvutika paumoyo wake akazunzikenso ku helo kwamuyaya ? ’ Maina ena asinthidwa . ( 1 Samueli 4 : 2 - 4 , 10 , 11 ) Aisiraeli anali kuganiza kuti kungotenga likasa ndi kupita nalo kunkhondo , ndiye kuti Yehova adzawathandiza ndi kuwateteza . Ayuda ambili anali kuuzonda ngako msonkho umenewu , cifukwa unali kuonetsa kuti iwo ali pansi pa ulamulilo wa Aroma . Koma ndinaganizila mmene Yehova alili wodekha ndi wololela kwa atumiki ake . N’cifukwa ciani kupanga zosankha tili okwiya kapena tili na nkhawa n’koopsa ? Iye anakondwela kwambili kuti anayesetsa kupezeka pa msonkhanowo . ( b ) Kodi mpesa za m’fanizo la Yesu ziimila ciani ? Nanga n’cifukwa ciani kuyelekezela mwanjila imeneyi n’koyenelela ? 4 : 6 , 7 ) Komanso cifukwa ca kudzipeleka kwathu kwa Yehova , tili “ pa mtendele ndi Mulungu , ” kapena kuti pa ubale wabwino na iye . — Aroma 5 : 1 . Muziyamikila Mwai Wanu Wogwila Nchito ndi Yehova , 10 / 15 M’kupita kwa nthawi , abale anathandizidwa kuwongolela maganizo awo olakwika pa nkhani ya cikwati , amene anacitsa kuti M’bale Diehl ndi mkazi wake acitilidwe zinthu mopanda cilungamo , ndipo iye anapatsidwanso mautumiki amene anali nawo poyamba . 20 : 2 ) Conco , n’zosavuta kudziŵa amene anali mnzake weniweni wa munthu womenyedwayo . Tiyeni tione zimene zinacitikila mtumwi Paulo . Komanso , bwelani kwa Yesu kuti akuphunzitseni coonadi cimene cingakutetezeni mofanana ndi mmene nkhuku imatetezela ana ake . Muyenela kuwapewa mwamsanga ! Mfundo ni yakuti : Pophunzitsa ana anu , osaseŵenzetsa njila imodzi - modzi nthawi zonse . N’cifukwa ciani tiyenela kusinkhasinkha pa zimene timaphunzila za Yehova monga Mfumu Davide ? Ndiyeno potsilizila pake , Atate wathu wa kumwamba amene ndi wacikondi adzakhala “ zinthu zonse kwa aliyense . ” — 1 Akor . MBILI : ATATE ANALI MSILAMU NDIPO AMAI ANALI MYUDA ( 1 Tim . 2 : 3,4 ) Lemba la Chivumbulutso 7 : 9 limanena kuti olambila Mulungu ndi ocokela “ m’dziko lililonse , fuko lililonse , mtundu uliwonse , ndi cinenelo ciliconse . ” Nthawi zonse ndinali kufuna kukondweletsa Mulungu . 5 : 11 ) — July - August , tsamba 4 . Iwo anali ngati alonda . Musakhumudwe ndi Zolakwa za Ena , June Georg Kayser anapita kunkhondo monga msilikali . Koma anabwelela kunyumba ali mtumiki wa Mulungu . Ndili ndi zifukwa zokwanila zokhalila wosangalala cifukwa kwa ine , kuyandikila kwa Mulungu ndi cinthu cabwino . — Yosimbidwa ndi Sarah Maiga . M’Ciheberi , liu loyambalo ni asher . ( Aroma 13 : 10 ) N’zosadabwitsa kuti Baibo imagogomeza kufunika kwa cikondi cifukwa “ Mulungu ndiye cikondi . ” ( 1 Yoh . M’kalata yake kwa Timoteyo , Mtumwi Paulo analemba kuti Akristu ayenela kusamalila a m’banja lao . Conco , atsogoleli acipembedzo sitiwapatsa ulemu wapadela , koma timawaona monga anthu ena onse . Msonkhano umenewo unasintha umoyo wanga . Pitilizani kufufuza mwakhama coonadi ca m’Baibo . Dzikoli likadzawonongedwa , aliyense kumwamba ndi padziko lapansi adzaona kuti Mulungu wacitadi cilungamo . Muzikambilana nawo nkhani zauzimu m’zocita zanu za tsiku ndi tsiku . Iye anangoniyang’anitsitsa mwaukali na kukamba kuti , “ Ni yokhoma ! ” Mlongo Anita amene lomba ali m’zaka za m’ma 70 , anali kukaikila ngako ngati angakwanitse . ‘ Kufunafuna coyamba cilungamo ca Mulungu ’ kumaphatikizapo kuona udindo wosamalila banja mmene Yehova amauonela . Ndipo pamene Yesu anawauza kuti aleke kuweluza ena , anawauzanso kuti : “ Kuti inunso musaweluzidwe , pakuti ciweluzo cimene mukuweluza naco ena inunso mudzaweluzidwa naco . ” — Mateyu 6 : 31 – 7 : 2 . Ndiyeno , ‘ inabala zipatso kuwilikiza maulendo 100 . ’ Ndinapemphela kwa Mulungu kuti andipatse nzelu , kenako ndinafufuza za nkhaniyi m’zofalitsa zathu . Mu mpingo wathu wa ku London , munali atumiki ambili a pa Beteli . Si udindo wathu kuweluza anthu a m’gawo lathu kapena a mumpingo Kuti tipambane pa nkhondo yathu yauzimu , sitifunika kudzidalila , koma tifunika kudalila Yehova . Billie Nichols na mkazi wake anali ena mwa anthu amene n’nabatizika nawo . Kutalika kwa nthawi imene tinakhala pamzele ndi kutentha kwa dzuŵa zinalibe kanthu kwa io . ” Tinali kuphunzila Baibo ndi acicepele ambili acikigizi amene anali kucita maphunzilo awo pa makoleji a m’delalo . Cifukwa ca mau a pa lembali , anthu ena amakamba kuti popeza tonse ndise ocimwa , sitiyenela kumuimba mlandu munthu akacita cigololo . Cinanso , Ababulo anali kunyoza Ayuda , pamodzi na Mulungu wawo , Yehova . ( Sal . Kodi Mulungu Amakuŵelengelani ? Mu 36 C.E . , ophunzila a Yesu anayamba kulalikila kwa anthu a mitundu yonse . Akamacita zimenezi , amaonetsa kuti makhalidwe apamwamba a Yehova monga kukhala oona mtima ni ofunika kwambili kwa iwo kuposa zinthu za kuthupi . — Miyambo 12 : 24 ; Aefeso 4 : 28 . Wophunzila Yakobo analemba kuti : “ Ngati wina sapunthwa pa mau , ameneyo ndi munthu wangwilo , ndipo akhoza kulamulilanso thupi lake lonse . ” Panopa , Baibulo la Dziko Latsopano , lathunthu kapena mbali yake cabe , likupezeka m’zinenelo zoposa 130 . M’bale Joseph F . Rutherford ataona kuti ambili amene analipo anali anthu a ku Poland anakhudzidwa kwambili cakuti anawauza kuti : “ Yehova wakubweletsani kuno ku France kuti muphunzile coonadi . Mlongo wacicepele dzina lake Brittney anafotokoza kuti : “ Kulambila kwa pabanja kwandithandiza kuyandikila kwambili makolo anga . Pokonzekela msonkhanowo , panafunika kukumbidwa mfolo wa mamita 400 kuti mupite mapaipi a gasi opita ku khicheni . Khalani ofunitsitsa kuleka kucita zinthu zimene zingakulepheletseni kukonda Ufumu wa Mulungu ndi mtima wanu wonse . Cikondi cimene Yehova amaonetsa anthu ake n’cosatha . Nanga bwanji za a “ nkhosa zina ” ? — Yoh . 10 : 16 . Komanso , Nowa anakwanitsa kusamalila udindo wake monga mutu wa banja cifukwa codalilanso nzelu za Mulungu . ( 1 Pet . 4 : 4 ) Angasonkhezelenso abululu athu amene amatikonda kuti azitiletsa kupita ku misonkhano . ( Mat . Conco mofanana ndi dalaivala amene tachula m’citsanzo cija , yemwe amaonetsetsa kuti wathila mafuta m’galimoto yake , akulu amafunika ‘ kutsimikizila kuti zinthu zofunika kwambili ndi ziti . ’ ( Afil . ( Mac . 11 : 28 , 29 ) Mtumwi Paulo ndi Petulo analimbikitsa Akhristu kuti azicelezana . Komabe , iye anapemphela kuti adziŵe mmene angathandizile anzake amene anakhudzidwa na vutoli . Izi zinapeleka mwayi wakuti anthu ena adziŵe zambili za Cikhiristu . 19 : 20 . Abale na alongo amene akhala kumidzi yakutali ndi mzinda wa Suva , likulu la dziko la Fiji , amalalikila uthenga wabwino kwa aliyense Ngati mufuna kuloŵa mu cikwati , pezani munthu amene mudzakonda kwambili . Komabe , ponena za ophunzila amenewo , Yesu anati : “ Mai anga ndi abale anga ndi awa amene amamvetsela mau a Mulungu ndi kuwacita . ” M’mau ake oyamba , Lefèvre anafotokoza kuti anamasulila mabuku a Uthenga Wabwino m’Cifulenchi kuti “ anthu wamba ” a m’chechi cawo “ amveleko uthenga wa coonadi mofanana ndi anthu amene anali kuŵelenga Baibo m’Cilatini . ” Izi zionetsa kuti Yosefe anali atakukila ku Yerusalemu camanje - manje kucoka ku Arimateya , * ndipo m’mandamo anali kufuna kuti aziikamo anthu a m’banja lake . Ndipo zimenezi zimakhala zopindulitsa kwa acibale athu kaya amatumikila Yehova kapena ai . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana funso imeneyi . Yehova wathandizanso anthu ake kuteteza ndi kulembetsa mwalamulo nchito yolalikila uthenga wabwino . Ganizilani zimene zinacitika usiku wakuti maŵa Yesu aphedwa . Mkazi wanga limodzi ndi anthu ena amandiyamikila kaamba ka kuyesetsa kwanga . Zekariya ayenela kuti anacita mantha kwambili ataona kuti mkaziyo afuna kutuluka m’ciwiyaco . ( Mat . 4 : 1 - 10 ) Komanso Ufumu wa Mulungu utakhazikitsidwa mu 1914 , Satana anapita “ kukacita nkhondo ” ndi otsalila odzozedwa . ( Chiv . Mwa mau andakatulo , wamasalimo analosela kuti ‘ mivi ya Mfumu yakuthwa idzalasa mitima ya adani a mfumu , ’ ndipo ‘ mitundu ya anthu idzagwa pamapazi ake . ’ Ndagwilitsila nchito maluso anga amene Yehova anandipatsa mwanjila imene sindikanatelo ndikanasankha nchito yakuthupi . ” Nanunso mungaphunzitse ana anu mwa citsanzo canu cabwino . Baibo imati : “ Kunena za kumwamba , kumwamba ndi kwa Yehova , Koma dziko lapansi analipeleka kwa ana a anthu . ” Malangizo anu acikondi adzathandiza ana anu kukula bwino ndi kukhala anthu okhwima , odalilika , ndi ocita zinthu moyenela . ( Aheberi 10 : 24 , 25 ) Mulungu amafuna kuti anthu amene amamulambila azisonkhana monga gulu . Kodi mavuto amatikhudza bwanji ? Koma m’modzi wa mamembala a gululo anathamanga n’kundiuza kuti ndibisale cifukwa gululo linali ndi colinga cakuti lindiphe . Iye anali na maganizo monga a mtumwi Paulo . ( Mac . Mofananamo Paulo atafunsa kuti “ Ndani adzandipulumutse ? ” Kodi Yobu anakumana ndi ziyeso zotani pamene anali wolemela komanso pamene anali wosauka ? 6 : 10 ; Yobu 31 : 32 . Akulu atam’patsa uphungu na kumuthandiza kukhalanso na cikumbumtima coyela , iye anati : “ N’napeza mpumulo . Uthenga wake unali wakuti io ayenela ‘ kukhalabe maso ’ kuti asataye mphoto yao ya mtengo wapatali . Koma Atate wathu wacikondi watilola kukhala “ anchito anzake . ” Mwakutelo , timaonetsa kuti timakonda Mulungu komanso anthu ena . Mofananamo , Yehova , Atate wathu wakumwamba amatikonda . Ndinakulila ku dela kumene kunali mavuto azacuma mumzinda wa Montreal . Olo kuti Yakobo anali kukhala na anthu amaganizo “ akuthupi , ” iye anali munthu wauzimu . Acibale athu sanakondwele pamene tinakhala a Mboni , cakuti atate ake Gwen anasiya kukamba ndi Gwen kwa zaka 6 . ( Mat . 24 : 42 ) Kuti ticite zimenezi , tiyenela kupewa zinthu zimene zingatilepheletse kukhala maso kuti tisazindikile kubwela kwa Yesu . Kuzindikila mwa njila imeneyo kungacepetse mkwiyo ndi kutithandiza “ kunyalanyaza colakwa . ” ( Miy . Mungatengele bwanji citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wolimba mtima ? Kodi mumacitila cifundo abale anu mocokela pansi pamtima ? Koma pamene tonse tinali kukula , tinali kufunitsitsa kuti kuvina kudzakhale nchito yathu . Koma moyo wanga uliko bwino tsopano cifukwa nimadzipeleka kwambili kutumikila ena . Musaiŵale kuti nzelu za anthu na njila zawo zolelela ana zimasiyana - siyana malinga ndi cikhalidwe ndiponso zimasintha m’kupita kwa nthawi . Komabe , cifukwa ca kukula kwa nchito panali kufunika anchito ambili ndiponso anafunika kugwila nchitoyi maola ambili . Ganizilani za m’bale John na mlongo Judith . Kwa zaka 30 zapitazi , iwo akhala akutumikila m’maiko osiyana - siyana . Iye ni wokhulupilika , wodalilika , ndipo sanama . Ndi kupanda nzelu kukangana ndi ampatuko kaya pamaso m’pamaso , pa webusaiti yao , kapena mwanjila ina iliyonse . Ndani anaona Yesu woukitsidwayo ? 30 Umoyo Wosalila Zambili Umabweletsa Cimwemwe Sin’nakayikile kuti n’nali kuphunzila coonadi . Motelo , ophunzila onse a Kristu ayenela kulalikila , kaya akuyembekezela kukalamulila kumwamba kapena kudzakhala padziko lapansi . — Mac . 10 : 42 . Iye anafotokoza kuti : “ Ndinafunsa abale ndi alongo kumene ndingazigula zakudya zochipa . SARA anali ataimilila pakati m’cipinda akuyang’ana uku na uku . Kodi Yehova amakamba nanu bwanji panokha kupyolela m’Mau ake ? M’malomwake Baibulo limeneli ndi limene anagwilitsila nchito pomasulila Baibulo lochedwa King James Version . — Ŵelengani 2 Timoteyo 2 : 9 . Kodi atumiki othandiza amathandiza bwanji kuti mpingo ukhale wogwilizana ? ( Agalatiya 6 : 5 ) Komabe , akulu angakambilane naye malangizo a Yehova kuti am’thandize kusankha mwanzelu . Iye anakamba kuti ni wa Mboni za Yehova ndipo afuna kutiuza uthenga wofunika kwambili . Tiyeni tikambilane mfundo zitatu zimodzi - modzi zimene zinatsogolela bungwe lolamulila m’zaka 100 zoyambilila . Yosefe anauza wopelekela cikho kuti nthambi zitatuzo zinali kuimila masiku atatu . 9 : 23 ) Kucita zimenezi kwakhala na zotulukapo zabwino ngako . Yesu anapitiliza kuti : “ Nthawi idzafika , ndipo ndi yomwe ino , pamene olambila oona adzalambila Atate motsogoleledwa ndi mzimu ndi coonadi , pakuti Atate amafuna otelowo azimulambila . ” Mgwilizanitsi wa bungwe la akulu mumpingo wawo anati : “ Iye ni mmodzi mwa abale ofatsa kwambili . ” Nanga bwanji aja amene anali kukhala m’matauni aang’ono ndi kumidzi ? Eduardo anali kuganizila mau amene timaŵelenga pa 1 Akorinto 7 : 28 . Mauwo amati , “ Oloŵa m’banja adzakhala ndi nsautso m’thupi mwawo . ” Cikondi ni khalidwe lalikulu kwambili pa makhalidwe onse . ( 1 Akor . Baibo inakambilatu kuti “ khamu lalikulu la anthu , limene palibe munthu aliyense amene anatha kuliŵelenga , locokela m’dziko lililonse , fuko lililonse , mtundu uliwonse , ndi cinenelo ciliconse ” lidzafuula kuti : “ Cipulumutso cathu cacokela kwa Mulungu wathu , amene wakhala pampando wacifumu , ndi kwa Mwanawankhosa . ” ( Chiv . 7 : 9 , 10 ) N’kosangalatsa cotani nanga ! Mwinanso timakonda kufotokoza zinthu mwa njila yakuti ciyamikilo cibwele kwambili kwa ife kuposa ena pa zimene zakwanilitsidwa , ngakhale kuti enanso anaikapo maganizo awo . Apanso Yesu anapeleka citsanzo cabwino . Komabe , kunyada kungaononge ubwenzi wathu ndi anthu ena ndiponso ndi Yehova . Kodi Aisiraeli anali kufunika kucita ciani kuti Yehova apitilize kuwadalitsa ? 11 : 35 ) Iye adzaika ena mwa io “ kukhala akalonga padziko lonse lapansi . ” Dzina lakuti Satana limatanthauza “ Wotsutsa , ” kuonetsa kuti mngelo woipayu sacilikiza ulamulilo wa Mulungu koma amadana nawo ndi kulimbana nawo mwamphamvu . Potsiliza fanizo lake , Yesu anakamba kuti mwini munda uja anatumiza mwana wake wokondedwa , amenenso anali wolandila coloŵa . Mfumu Yosiya , mdzukulutubzi wa Hezekiya , nayenso anasunga malamulo a Yehova “ ndi mtima wake wonse . ” Kodi zipembedzo zonse zimatsogolela anthu kwa Mulungu woona ? Tingatsanzile bwanji Yehova ndi Kristu ? Colinga ca Mlengi wathu poyamba cinali cakuti anthu akhale ndi moyo wosatha padziko lapansi . 127 : 3 ) Adamu na Hava akanamvela Mulungu , akanasangalala na umoyo wa banja kwamuyaya . ( Yakobo 1 : 14 , 15 ) Anthu akayamba kucita zinthu motsatila zilakolako zoipa kapena kugonja ku zilakolako zoipa , angakumane ndi mavuto . Tinathaŵila ku tauni ya Schladming . Popeza mbeu imeneyo idzaphwanya mutu wa njoka , kapena kuti ‘ kuononga ’ colengedwa cauzimu , Satana Mdyelekezi , ndiye kuti mbeu imeneyo iyenela kukhala colengedwa cauzimu . Panthawi ina , mkazi wamasiye ndiponso wosauka wa ku Zarefati , tauni ya m’mbali mwa nyanja m’cigawo ca Foinike , anaceleza mneneli Eliya . Ndinaŵayankha kuti : “ Mboni za Yehova za ku America nazonso zikaŵelenga lembali zimadziŵa kuti likuchula likulu lao . ” Mkati mwa dzikolo muli cipululu cacikulu kupitilila hafu ya dziko la America , ndipo munali kukhala anthu ocepa . Fanizo la kapolo wokhulupilika , la anamwali 10 , ndi la matalente , onsewa amakhudza otsatila ake odzozedwa . Panthawiyo m’dzikolo munali Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse . Ndipo m’nkhani yotsatila , tidzakambilana njila zinai zimene tingaonetsele kuti timakonda Mulungu . Fotokozani zitsanzo zina za anthu a m’Baibo amene anali odziletsa ndi amene anali osadziletsa . 46 : 1 . Mwacitsanzo , ngati mwamuna angapatse mkazi mphatso pa cifukwa cosadziŵika bwino , mkaziyo angaganize kuti mphatsoyo ni cizindikilo cakuti afuna kum’dziŵa bwino . Davide atamuona , anamvetsa cifukwa cake asilikali a Isiraeli anali kumuopa . Anali cimunthu cacikulu ndi coopsa , kapena kuti ciphona . James Mantz Ndasangalala kuti mwabwela lelo . Ndili ndi funso . PA CIKUTO : Akulalikila atagwila Baibulo m’manja , mumzinda wokongola wocedwa Grindelwald , ndipo mapili amene akuonekela ca kumbuyo amacedwa Bernese Alps ( Onani mau a munsi . ) ( b ) N’cifukwa ciani akulu ena amalephela kuphunzitsa ena ? Nsanja ya Mlonda iyi ionetsa zimene Baibo imakamba ponena za angelo , na mmene amakhudzila umoyo wathu . GANIZILANI mmene mukanamvelela kuona Yesu Kristu ‘ akukondwela kwambili mwa mzimu woyela . ’ Mukamafuna - funa Ufumu coyamba , mudzakhala ndi mipata yambili ya utumiki . Koma , mungadzifunse kuti , ‘ Kodi kuvutika ndi cisalungamo zinali mbali ya colingaco ? ’ — Ŵelengani Deuteronomo 32 : 4 , 5 . Kodi Malemba amavomeleza motani mfundo imeneyi ? “ Naphunzila kuti ngati ugwila nchito molimbika , umakhala wacimwemwe komanso wokhutila . Kodi kuganizila zimenezi kumakukhudzani bwanji ? Kacisi wa Ayuda anali nyumba yeniyeni yomangidwa pamalo ena ake . M’busayo ndi mtsikana wake , anayamikilanso zinthu zina kuonjezela pa maonekedwe ao . Ndi magazi okha a Yesu amene adzacititsa kuti macimo athu akhululukidwe , ndi kuti tikapeze moyo wosatha . — Yoh . ( c ) Tidzakambilana ciani m’nkhani ino ? Iye anandipatsa mabuku angapo ofotokoza Baibulo . Iwo sadziŵa mmene anthu amamvelela , zimene amasoŵa , ndi zofooka zao . Baibulo imafotokoza kuti Yesu anadzipeleka , kuphatikizapo kupeleka moyo wake , kuti athandize ena . Mwina cifukwa ca zinthu zinayi izi : ( 1 ) amene anakupatsani mphatsoyo , ( 2 ) cifukwa cimene anakupatsilani , ( 3 ) zimene anatailapo kuti akupatseni mphatsoyo , ndi ( 4 ) ngati mphatsoyo inakwanilitsa zosoŵa zanu . ( 2 Timoteyo 3 : 1 ; Maliko 13 : 19 ) Komanso Satana ndi ziŵanda zake anacotsedwa kumwamba ndi kuponyedwa kudziko lapansi . Zimenezi zinacititsa kuti anthufe tiyambe kuvutika kwambili . N’cifukwa ciani lemba la Aroma 5 : 12 n’lofunika kwa Mboni za Yehova ? ( Miy . 11 : 2 , 20 ) Anthu ambili amavala zovala zosambila zoonetsa thupi , koma ife amene titumikila Yehova timaganizila zimene zingalemekeze Mulungu wathu woyela amene timakonda . Iwo salandilanso malipilo alionse . ” Kodi mukanaonetsa kufatsa ? Timayamikila kwambili Nowa ndi mkazi wake , kuphatikizapo ana ake aamuna ndi akazi ao cifukwa tili ndi moyo kaamba ka kukhulupilika kwao ndi kucita zinthu zokondweletsa Yehova . Mwina tingafunse kuti , ‘ Kodi cikondi caciphamaso n’cikondidi ? ’ Yehova wapatsa makolo udindo wofunika kwambili . Ine , amayi anga , na mng’ono wanga Grigory , anaticotsa ku Ukraine . Bungwe Lolamulila masiku ano lili ndi udindo waukulu woyang’anila nchito yolalikila padziko lonse imene ikugwilidwa ndi ofalitsa oposa 8 miliyoni . ‘ Kuyambila pamene anali wakhanda , ’ Timoteyo anaphunzitsidwa kukonda Malemba oyela Aciheberi . M’malo mom’dzudzula , Yesu mokoma mtima anati : “ Mwanawe , cikhulupililo cako cakucilitsa . Kodi mungadzipeleke kuti mutumikile Yehova mu utumiki wa nthawi zonse ? Mu February 2012 , n’nagwa na kuthyoka fupa la m’ciuno , ndipo zinaonekelatu kuti nifunika wina wonisamalila . 12 : 22 , 25 ) Ganizilani zimene zinacitikila Dannykarl , amene anacoka ku Philippines n’kukakhala ku Japan . Cifukwa ca cikhulupililo , Mose anazindikila kuti ‘ zosangalatsa zaucimo ’ zinali zosakhalitsa . Natani anapeleka uthenga wa Mulungu kwa Davide . M’ndakatulo imeneyo , anaunikila lonjezo lakuti anthu adzabwezeletsedwa ku moyo wamuyaya padziko lapansi , pokamba kuti : “ Panthawiyo , dziko lonse lapansi lidzakhala paradaiso . ” 10 , 11 . ( a ) Kodi acicepele ambili amakumana na vuto lanji kusukulu ? Koma tikabwelako , timadziŵa kuti umoyo udzakhalanso mmene unalili tisanapite . Ngati wocimwayo salapa , ayenela kucotsedwa mu mpingo pofuna kusungitsa ciyelo ca mpingo . ( 1 Akor . ( Mat . 2 : 1 - 3 , 13 ) Pofuna kuonetsetsa kuti khandalo laphedwa ndithu , iye analamula anthu kukapha ana onse aamuna m’Betelehemu ndi m’zigawo zake , kuyambila azaka ziŵili kutsika m’munsi . KUONA MTIMA , KULIMBIKA PA NCHITO Iwo akhala patsogolo pa nyumba ya kamangidwe ka kumudzi wacindebele . Ndipo salemekeza Mulungu mwa kuphunzitsa nzelu za anthu , kumenya nkhondo zimene amati ndi ‘ zopatulika , ’ ndi kucita ciwelewele . ( Sal . 106 : 35 - 39 ) Conco , popeza kuti io sanakhulupilike kwa Mulungu , Yesu anawauza kuti : “ Tsopano tamvelani ! Angacite izi mwa kum’phunzitsa na kum’patsa cibalo . Sara anakhalabe wokhulupilika kwa mwamuna wake , olo kuti m’nyumba yacifumu ya Farao munali zinthu zambili zokopa ya March 2007 , mapeji 10 - 12 . Ndiye cifukwa cake m’busayo anali kumuona kuti ndi wapadela “ monga duwa pakati pa zitsamba zaminga . ” Yehova amafuna kuti tizipanga tokha zosankha , ndipo zimenezi zili na ubwino wake . Conco , ndinapita kukauza sisitele wamkulu kuti ndifuna kucoka . Zimene zinacitika pa Pentekosite mu 33 C.E . , zinatsimikizila kuti Yehova analandila mokondwela nsembe yangwilo , ya mtengo wapatali ya Yesu yophimba macimo . ( Aheb . Ngati anthu ndi angelo sangadziŵe zoona pankhaniyi , n’zosatheka padziko lapansi kukhala mgwilizano ndi mtendele weni - weni . Komabe , tifunikanso kudziŵa kuti kungokhulupilila kuti Yesu aliko sikokwanila . Lamulo la Mulungu lakuti , “ tuluka m’dziko lako ndi pakati pa abale ako ” liyenela kuti linali lovuta kwa Sara . TSAMBA 11 • NYIMBO : 97 , 96 Iwo amaika maganizo awo onse pa kudziunjikila cuma kapena kuciteteza . cimatithandiza bwanji kukhala olimbikitsa mgwilizano ? ( b ) Nanga Mose anapulumuka bwanji ali mwana ? Ndipo Yehova anacitanji kwa anthu ake ? Amene amafuna kupatsidwa ulemu , m’patseni ulemu wake . ” — Aroma 13 : 1 , 7 . Ise Akhristu , ndise a m’nyumba ya Mulungu . ( Luka 18 : 27 ) Mlengi wa cilengedwe conse akufuna kuti anthu am’peze ndi kumudziŵa . Kutumikila monga mpainiya wapadela kumaphatikizapo ciani ? ( Aef . 4 : 29 ) Tikamauza ena za Ufumu wa Mulungu , mau athu ayenela kukhala okoma ngati kuti ‘ tawathila mcele . ’ ( Akol . Kugalukila boma kapena masitalaka pa nchito zikucitika kaŵili - kaŵili ngakhale masiku ano . Conco , acinyamata amene akutumikila Yehova amaona kuti pamafunika khama kwambili kuti apewe mzimu umenewu n’kuyamba kuona zinthu mmene Mulungu amazionela . Atumwi anadziŵa kuti kuuka kwa Yesu kunali kosiyana ndi kwa anthu akale amene anaukitsidwapo . ▪ Yehova Adzakucilikizani 5 : 1 , 7 - 9 ) N’cifukwa ciani Yehova anaonetsa mneneli wake masomphenya ocititsa cidwi amenewa ? Ndiye kuti mukulola Yehova kukuumbani na kukulangani kuti mupindule . — Miy . Mwakutelo , mudzakhala pa mzela wa atumiki a Mulungu okhulupilika ambili . Ganizilani mmene Yosefe anamvelela pamene anthu ocokela kwa Farao anabwela kudzamuitana . Kwa zaka zambili , anthu anali kusindikiza mabuku pogwilitsila nchito makina amene Johannes Gutenberg anapanga mu 1450 . Anthu odzikonda otelo sakhala na cimwemwe ceni - ceni . Koma mofanana ndi wamalonda uja , iyenso anali wofunitsitsa kugulitsa “ zinthu zonse ” ndi kugula mundawo . Iye akudzifunsa kuti : ‘ N’cifukwa ciani ndikuvutika ndi nchito yaukapolo imeneyi ? Nthawi zina , n’nali kulaka - laka kukhala na manja opanga amene anganithandize kucita ciliconse cimene nafuna . 3 : 15 - 18 ; 4 : 1 . Conco , ngati mwafooka cifukwa ca mavuto ndipo muli na nkhawa , musatalikilane naye Yehova . Ngati ndimwe mmodzi wa abale okondedwa amenewa , mwacionekele mumakondwela na udindo wanu watsopano . Panthawi ina , atsogoleli osiyana - siyana amphamvu anayesetsa kuletsa nchito yomasulila Baibo kuti anthu wamba asakhale na mwayi woiŵelenga . Kumbukilani kuti iye analonjeza kuti sadzatisiya . — Aheb . Tili pa ubale wabwino na Yehova cifukwa tinamudziŵa ndipo timatsatila Mau ake pa umoyo wathu . ( Luka 16 : 10 ) Kodi mabwenzi a Yehova amenewa amamvela bwanji akaganizila zopeleka zimene amacita ? ( Aheberi 6 : 1 , 2 ) Mwacitsanzo , kuphunzila maulosi a m’Baibulo amene anakwanilitsidwa kale kudzakuthandizani kuonjezela ndi kulimbitsa cikhulupililo canu . Ciyembekezo cathu si copanda maziko , koma n’cozikidwa zolimba pa umboni wa m’Malemba umene umaticititsa kukhalabe maso ndi kuyembekezela mapeto a dziko loipali . Komabe , mwa kugwilitsila nchito lamulo lakuti “ moyo kulipila moyo , ” Mulungu anaonetsa cilungamo ndi kucititsa kuti anthu omvela akhalenso ndi ciyembekezo ca moyo wosatha . 12 : 1 ) Zimenezi ndi zimene Yesu adzacita moimilako Mulungu , ndipo zimafotokozedwanso pa Chivumbulutso 19 : 11 - 21 . 24 : 30 ) Mau amenewa akusonyeza kuti kubwela kwake kudzakhala kosaonekela ndi maso . Kodi inunso mufuna kucita zimenezi ? Anali kuganizila kwambili za ciyembekezo cake cokakhala m’dziko latsopano lolamulidwa na Mesiya . Kuphunzitsa coonadi ca m’Malemba kudzathandiza kuti ife ndi aja otimvela tidzapulumuke . — 1 Tim . Petulo anagwela mumsampha woopa anthu . ya Chichewa ya September 2009 . Timalimbitsa cikhulupililo cathu ngati timapempha mzimu woyela , timaphunzila Baibulo tsiku lililonse , timapezeka pa misonkhano , timaceza ndi abale ndi alongo athu , ndiponso ngati timalalikila uthenga wabwino Ndi Amphamvu ” Baibo imafotokoza kuti makolo athu oyambilila , Adamu na Hava , analengedwa angwilo . Iwo anali na ciyembekezo cosangalala kwamuyaya na moyo m’paradaiso padziko lapansi , pamodzi na ana awo amene anali kudzakhala nawo m’tsogolo . N’zoonekelatu kuti ngati ophunzila Baibulo asintha kuti akondweletse Mulungu , Iye adzawayandikila ndi kuwaumba kuti akhale ziwiya zolemekezeka . Poyamba , Baibulo linalembedwa m’Ciheberi , m’Ciaramu , ndi m’Cigiriki . Kodi Yehova anapeleka ciweluzo cotani kwa Adamu ndi Hava ? Mungasinkhesinkhenso nkhani zimene zimapezeka mu Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani ! Dzina lasintha . ( Chivumbulutso 21 : 5 ) Nimatsimikizila kuti lonjezo limeneli lidzakwanilitsika nikaganizila zimene Yesu anacita pamene anali pano padziko . Potonthoza ena , tingagwilitsile nchito bwanji Yeremiya 29 : 11 ? ( Ŵelengani Salimo 130 : 3 . ) Koma m’maiko ena , n’kofala kwambili . Panangopita caka cimodzi mwana wawo wamkazi n’kumwalila . Kodi tingathandize bwanji Akristu okalamba ndi odwala kuti azitengako mbali pakulambila koona ? Anthu ambili masiku ano amafuna kukhala odziŵika kwa ena m’dziko loipali . ( Mat . 9 : 37 ; 24 : 14 ) Onani mmene mau ake akwanilitsidwila mocititsa cidwi m’dela la Transcarpathia , ku Ukraine . Mungadziŵiletu zakudya zakumeneko . Zimenezi zinandidetsa nkhawa . N’cifukwa ciani tifunika kukamba zoona nthawi zonse ? ( b ) Kodi Mulungu amawathandiza bwanji makolo kukwanilitsa udindo wawo ? “ Mwana angaphunzile makhalidwe oipa panthawi iliyonse , kaya ni pa foni kapena pa tabuleti . ( Zek . 4 : 1 - 3 , 14 ) Caciŵili , mboni ziŵili zimenezi zikufotokozedwa kuti zikucita zizindikilo zofanana ndi zimene Mose ndi Eliya anacita . — Yelekezelani Chivumbulutso 11 : 5 , 6 ndi Numeri 16 : 1 - 7 , 28 - 35 ndiponso 1 Mafumu 17 : 1 ; 18 : 41 - 45 . Cimatiŵaŵanso tikagonja ku zizoloŵezi zoipa zathupi , kapenanso tikalephela kuthetsa nsanje . Koma Yehova salakwitsa ciliconse . Kodi ali na cidziŵitso cofikapo moti angadzipeleke moyenela ? Mlongoyo angaganizile mfundo zofunika za m’Baibo monga mfundo yakuti tifunika kumvela Mulungu ndi yakuti tifunika kupanga ophunzila . ( Mat . 28 : 19 , 20 ; Mac . Panthawiyo , Chechi ya Katolika pamodzi ndi akatswili a zacipembedzo , anali kuletsa kuti Baibo imasulidwe m’zinenelo zofala . Kuti tipambane pa nkhondo yoteteza maganizo athu , tifunika kuzindikila kuopsa kwa mauthenga osoceletsa a Satana ndi kupeza njila zodzitetezela . Yehova anali kufuna kuti pa dziko lapansi pazicitika zinthu zabwino , osati zoipa zimene timaona kaŵili - kaŵili masiku ano . Atawasunga kwa masiku aŵili , mkulu wa asilikali anatumila foni bwana wake na kum’funsa zimene angawacite abalewo . Mwacidziŵikile , podabwa mungafunse kuti , ‘ Kodi cinapangiwa na ciani ? ’ 3 : 9 ) Akristu ena ali ndi mwai wogwila nchito yomanga Nyumba za Misonkhano , Nyumba za Ufumu , ndi maofesi a nthambi . Nchito imeneyi ifanana ndi imene Nowa ndi Mose anagwila . Koma kodi nchito yathu ndi yotani ? Iwo anali kuyang’ana mwacidwi maboti akulu - akulu amene analandiwa , zikwangwani zoonetsa zithunzi za nkhondo na zinthu zina zimene anatenga mu kacisi ku Yerusalemu . Timacita izi mwa kusunga malamulo ake . Anthu ena amaganiza kuti dzina limeneli linali kugwilitsidwa nchito m’nthawi imeneyo cabe . TSAMBA 9 • NYIMBO : 54 , 43 Nanga tingaphunzilepo ciani pa cikhulupililo ca mnyamata amene ananzunzidwa ndi kukanidwa ndi anthu a m’banja lake ? ( 1 Yohane 2 : 15 , 16 ) Lemba la 1 Yohane 5 : 19 limati : “ Dziko lonse lili m’manja mwa woipayo . ” * Komanso , ganizilani cisangalalo cimene adzakhala naco akadzamvetsetsa mbali imene anacita pokwanilitsa colinga ca Yehova cokhudza mbeu yolonjezedwa . N’ciani cimene cionetsa kuti Petulo anaphunzila kucita zinthu mopanda tsankho ndi anthu onse ? Kodi anapatsiwa nchito yanji ? Komabe , iye anawonjezela kuti : “ Mothandizidwa ndi anthu ena , cisoni cimayamba kucepa pang’onopang’ono . ” Abusa oona acikhristu amalabadila modzicepetsa mau a Yesu akuti : “ Koma inu musamachulidwe kuti Rabi , cifukwa mphunzitsi wanu ndi mmodzi yekha , ndipo nonsenu ndinu abale . ( Yesaya 32 : 1 , 2 ) Pamene tiŵelenga ziyeneletso zimenezi , timaona kuti Yehova amatisamaliladi . ( Onani bokosi yakuti “ Anapeleka Thandizo Loyenela . ” ) Kuti titsanzile cikondi ca Mulungu tiyenela kuganizila mmene ena akumvelela . — 1 Akor . Ngati m’banja muli ana , iwo angayambe kuvutika maganizo , kukhumudwa , na kudzimva kuti ni osatetezeka komanso osoŵa cikondi . ( a ) Kodi mzimu wa Ayuda wotsutsa unamukhudza bwanji Paulo ? Ngati munthu wapha mnzake mwangozi , thandizo linalipo . Koma munthuyo anali kufunika kucitapo kanthu kuti athandizidwe . Zikakhala conco , mwamsanga tinali kufunika kuganiza zocita , kaya kupepesa na kucokapo kapena kuwalalikila mwacidule . Pa tsiku loyamba la msonkhanowo , azilongosi anga anali kunilembela mfundo za m’nkhani mosinthana - sinthana kuti nipindule na pulogilamu . Patangopita nthawi yocepa , tinazindikila kuti tinali kumvetsa molakwa mau ambili amene tinali kuphunzila . Paulo anayamba kuchula makhalidwewa ni mau akuti “ pakuti anthu adzakhala . . . Ine ndi Angela , tili na mlongo Etta Huth Kodi anacita zimenezi n’colinga cofuna kutigwilitsa mwala ? Iyai . Kodi Yehova waticitila zinthu zina ziti zimene zingatithandize kukhala na cimwemwe ? Muzitumikila mokondwela ngakhale kuti ena saona zimene mumacita . Kukumbukila mavuto amene anthu m’dela lathu apitamo , kumanithandiza kupitiliza kuwaonetsa cifundo . Pamene Mwana wa Yehova anabwela pa dziko , anapeleka citsanzo cabwino kwambili ca mmene tingalimbikitsile ena . Koma ngakhale iye asanabwele , atumiki a Yehova anali kudziŵa kuti kulimbikitsa ena n’kofunika . Ŵelengani Mateyu 6 : 28 - 30 . Yehova afuna kuti anthu onse apindule ndi dipo , kuphatikizapo aja amene anakhala ndi moyo dipo lisanalipilidwe . M’nkhani zoyambilila , taona umboni wakuti pemphelo n’lofunika kwambili osati polambila cabe kapena tikapanikizika maganizo . Nanga bwanji ngati ndinu wacicepele , ndipo muona kuti makolo anu acikhristu sakumvetsetsani kapena sakupatsani ufulu wokwanila ? Mosiyana na Yehova , alembi na Afarisi sanali kulemekeza moyo . ( Mateyu 15 : 14 ) Yesu sanagwilizane ndi atsogoleli acipembedzo amenewa ngakhale pang’ono . ( Yohane 1 : 46 ) Mukanakhalapo , kodi mukanaganiza kuti Natanayeli amakonda kukamba zoipa ponena za anthu ena , amaweluza ena , ndipo alibe cikhulupililo ? Umu si mmene Yesu anamuonela . Kuonjezela pamenepo , kaŵilikaŵili boma limaononga ndalama zambili pofuna kuonetsetsa kuti anthu akutsatila malamulo oletsa ziphuphu , koma zimenezi sizithandiza kwenikweni . Koposa izi , mphatso ya Mulungu ya nsembe ya Yesu , amene anatifela , ingacititse kuti tikalandile madalitso oculuka monga mmene taphunzilila pa Yohane 3 : 16 . Komabe , asayansi apeza kuti cifukwa ca mmene ma IUD amaseŵenzela , zimangocitika mosayembekezeka kuti mimba ikhale . Ngakhale kuti mana anali mphatso yocokela kwa Mulungu , sanali kupeleka moyo wosatha . ( Ŵelengani Luka 4 : 22 . ) Ngakhale kuti Sara sapeza ndalama zambili ngati mmene anali kucitila kale , iye tsopano akwanitsa kucita upainiya . 5 : 19 ) Nzika zonse zokhulupilika za Mfumu ziyenela kutengela citsanzo cake ndi kugonjela modzicepetsa ku ulamulilo wa Yehova m’zinthu zonse . A . Kuzunzidwa kwa Mboni za Yehova kunacititsa kuti ciŵelengelo cawo ciwonjezeke ku Kyrgyzstan . 3 : 2 , 7 . Acinyamata oposa 60 pelesenti anayankha kuti amakhulupililadi kuti Yesu amayankha . Ngakhale kuti Atate wathu wa kumwamba alibe tsankho , nthawi zina iye amasankha atumiki ake okhulupilika ndi kuwakomela mtima . 119 : 18 ) Ndi njila zina ziti zimene mungagwilitsile nchito pothandiza wophunzila ? 1 : 8 - 10 . 5 : 10 ; Yak . 4 : 8 ) M’nkhani ino , tidzakambilana mavuto aŵili amene angacepetse cangu cathu potumikila Mulungu . Tidzakambilananso mmene kuseŵenzetsa mfundo za m’Baibo kungatithandizile kupilila mavuto amenewo . Pamene muŵelenga , musakhale cabe na colinga cofuna kutsiliza nkhaniyo . ( Mat . 24 : 36 ; 25 : 13 ) Koma tingathe kudziŵa “ nyengo ino , ” ndipo tikuidziŵa monga mmene Paulo anakambila . 16 : 7 ; Yoh . 6 : 44 . Kuganizila kwambili mapangano amenewa kudzatithandiza kumvetsetsa mmene cifunilo ca Mulungu cidzakwanilitsidwila . Kudzatithandizanso kuona kudalilika kwa Ufumu wa Mesiya . — Ŵelengani Aefeso 2 : 12 . Ni anthu ati amene ayenela kulemekezedwa ? Lamba imene asilikali aciroma anali kuvala inali ya tunsimbi topyapyala , tumene tunali kuteteza ciuno cake . N’nali kuopa kucita zinthu zoipa poganiza kuti ningakhumudwitse Yehova . Filip anati : “ Ninali kuphunzila ndi mnyamata wina dzina lake Michael . Mungauzeko mwamuna kapena mkazi wanu , wacibale , kapena mzanu wodalilika mmene mumvelela . Kodi ulosi wa pa Salimo 16 : 10 unakwanilitsika bwanji ? Nanga zimenezi zititsimikizila ciani ponena za lonjezo la kuuka kwa akufa ? Iye sanangokamba kuti : “ Tiyenela kupilila masautso ambili . ” Ndipo mipukutu ina yoyambilila ya Baibulo inapezeka m’mitsuko , m’zipinda zosungilamo zinthu , ndi m’mapanga . Komabe , iye anakana cifukwa anadziŵa kuti nchitoyo idzamulepheletsa kucita upainiya . Mwacionekele , Elisa sanadzimve kuti popeza kuti iye tsopano ndiye anali mtsogoleli anafunika kusintha zinthu mwamsanga . Zimenezi zikutanthauza kuti Yehova ndi amene anamuika kukhala Mfumu . Ngakhale n’conco , Baibo imakamba kuti “ lilime la anthu anzelu limacilitsa . ” Akwatile . ” ( 1 Akor . Tikulitse cidalilo mwa Yehova pamene ticitapo kanthu moyenelela . Popeza kuti banja lake linali kutali , anayamba kusungulumwa ndi kuyewa kunyumba . Kuti timveketse mfundo ya fanizoli , tingafunse kholo kuti , “ Kodi mungapeleke mwana wanu kwa munthu woipayo kuti am’patse cilango ? ” Kodi fanizo limeneli limatanthauza ciani ? Mwacitsanzo , ganizilani zimene zinacitika pa nthawi ya cakudya cothela cimene iye anadya na ophunzila ake . ( Aroma 15 : 4 ) Citsanzo cabwino ni nkhani ya Yosefe . 7 , 8 . ( a ) Kodi ophunzila a Yesu anaphunzilapo ciani pa pemphelo lake ? Ziwiya za seŵelo limeneli zinali zonyamula m’manja , ndipo linali lopanda zithunzi . Seŵelo limeneli linali ndi mbali zitatu , ndipo mbali iliyonse inali m’zinenelo zingapo . 144 : 15 . Limati agalu anali kunyambita magazi a mfumuyo . Cocitika cimeneci cinakwanilitsa mau amene Yehova anauza Ahabu kudzela mwa Eliya akuti : “ Pamalo amene agalu ananyambita magazi a Naboti , pomweponso agalu adzanyambita magazi ako , a iweyo . ” — 1 Mafumu 21 : 19 ; 22 : 19 - 22 , 34 - 38 . Koma amene anali ku mbali ya Yehova analonjezedwa kuti adzadalitsidwa . — Eks . Pamene Yehova anasankha Yoswa kuti atsogolele Aisiraeli , anauzanso Mose kuti “ umulimbikitse ndi kumulimbitsa . ” Zimene timacita tikakumana na ciyeso , kaya cacikulu kapena cacing’ono , zifunika kuonetsa kuti timafuna kukwanilitsa lonjezo lathu lakuti tidzatamanda Yehova “ tsiku ndi tsiku . ” ( Sal . ( Mateyu 4 : 4 ) Monga mmene cakudya cilili cofunika m’thupi lathu , kuphunzila za Mulungu n’kofunika kwambili . Pa nthawiyo , nkhondo imeneyi anali kuicha “ Nkhondo Yaikulu . ” Ndi vuto liti limene linabuka pakati pa Akristu oyambilila ? Ndipo n’ciani cinacitika patapita zaka zambili ? Caciŵili , ngati tikonda kucita zinthu m’mphamvu zathu , posapita nthawi , kapena m’kupita kwa nthawi , tidzayamba kukwesana ndi anzathu . Koma pamene Mulungu anawafufuza , anaona kuti mitima yawo inali yathunthu kwa iye . Mwina tingazindikile kuti afunikila thandizo kuti adziŵe bwino cinenelo . Kunena za tumabuku tumene tachula pamwambapa , m’bale wa ku America wa wazaka 19 anakamba kuti : “ Tumabuku utu twan’thandiza kwambili . Cifukwa cakuti Yonatani anali wokhulupilika kwa Yehova ndiponso anali wodzicepetsa . ( 1 Akorinto 15 : 26 ) Komabe , Mulungu ni wamuyaya . Conco makolo , muzikonda kuseŵenzetsa mafanizo powaphunzitsa . Iye anati : “ Ndatsegula pakamwa panga pamaso pa Yehova , ndipo sindingathe kubweza mau anga . ” N’cifukwa ciani tifuna kuti Yehova azitiphunzitsa ? Ndipo m’makhotiwo anali kuweluzilamo milandu ing’ono - ing’ono popanda Aroma kuloŵelelapo . Koma zinthu zimene timalakalaka n’zambili . Iye ndi alongo ake atatu amasamalila makolo ao okalamba , ndipo amai ao ali ndi matenda a muubongo . Iye ananifunsa ngati nidziŵa kuti Mulungu angacititse kuti nikhalenso na manja . Tsopano inuyo mufewetse nchito yoŵaŵa ya bambo anu ndi goli lawo lolemela limene anatisenzetsa , ndipo tidzakutumikilani . ” — 2 Mbiri 10 : 3 , 4 . Pa nkhani ya Hezekiya , tiphunzilapo mfundo yonena za mtima . Mwacitsanzo , panthawi ina , ine ndi anzanga tinali kuonelela filimu yoonetsa mmene kale anthu akuda anali kuvutitsidwila ku dziko la United States . ZINTHU ZONSE ni za Yehova ! N’zocititsa cidwi kwambili kuona nchito yaikulu yolalikila uthenga wabwino imene anthu a Yehova akugwila masiku ano otsiliza . Nthawi zina , tingasoŵe zinthu zakuthupi zofunikila pa umoyo . Mungapewe nkhawa zambili mwa kulabadila uphungu wa mtumwi Paulo , wakuti tizikhala ‘ okhutila ndi zimene tili nazo pa nthawi ino . ’ ( 1 Mbiri 28 : 9 ) Kuti timvetsetse cisamalilo cacikondi ca Mulungu , tiyeni tione mmene anacitila ndi Kaini . Koma n’napemphela kwa Mulungu , ndipo ananitonthoza . Idzalimbikitsanso aliyense wa ife kukhalabe nzika yokhulupilika ya Ufumu , ndiponso idzatilimbikitsa kusinkha - sinkha tanthauzo la lemba la caka ca 2014 . Boma likakweza misonkho , anthu amacitanso ziphuphu kwambili . Conco , sicinali cinthu canzelu Yosiya kukacita nkhondo ndi Neko . 28 : 19 ) Ndiponso timafuna ‘ kucitila onse zabwino , ’ makamaka abale athu ndi anzathu . — Agal . Izi ni zina mwa zinthu zambili - mbili zimene atumiki a Yehova amadzimana pom’tumikila . Ufumu wa Mulungu , umene Mfumu yake ni Yesu Khristu , udzalamulila mogwilizana na cifunilo ca Yehova , amene ni Mulungu wadongosolo . ( 1 Akor . 25 : 6 - 8 , 14 , 15 ; 2 Maf . “ Khulupilila mwa Ambuye Yesu ndipo udzapulumuka . ” — Machitidwe 16 : 31 . 12 : 9 , 10 . Bwanji ngati pakali pano mulibe maganizo ocita upainiya ? Okalamba ena ali ndi ana ambili pamene ena ali ndi mmodzi cabe . Cuma Camasiye : Mukhoza kulemba mu wilu yovomelezeka na boma kuti gulu la Mboni za Yehova lidzapatsidwe katundu wanu kapena ndalama zanu , inuyo mukadzamwalila . Nkhani ya Naboti timaimvetsa bwino kwambili masiku ano . M’pomveka kuti Baibo imaticenjeza kuti tifunika kupewa kupsa mtima , kukamba mau acipongwe , ndi kulalata . ( Aef . ( Luka 10 : 21 ; Yoh . 4 : 34 ) Mwina inunso muli ndi cimwemwe cifukwa cothandiza ena . Komabe , onani mmene mkazi wina dzina lake Ana amamvelela mwamuna wake akamuuza maganizo ake . 12 : 8 ) Koma mwina simukondwela na mmene amakupatsilani malangizowo . ( Aroma 8 : 38 , 39 ) “ Tikakhala ndi moyo , timakhalila moyo Yehova , ndipo tikafa , timafela Yehova . Adamu ayenela kuti anadya cipatso cimene mkazi wake , Hava , anamupatsa cifukwa cofuna kumukondweletsa . Abale ndi alongo athu , ngakhalenso anthu ena onse , afunika kuona kuti ndife oyeneleladi kuimila Mulungu wathu wolungama . ( 2 Mbiri 32 : 2 - 4 ) Koma kodi Yehova anawathandiza bwanji ? Kodi Nowa anaonetsa bwanji kuti anali wolimba mtima kwambili ? Iye amatithandiza kusintha kuti tikhale anthu abwino Kodi zimene zinacitikila Sebina zakuphunzitsani ciani zokhudza cilango ca Mulungu ? Koma amapitiliza kukambilana kuti athetse kusemphana maganizo . Mofanana ndi Yosefe , munthu aliyense wokonda kupemphela afunika kukhala wodzicepetsa ndi kudalila Mulungu kuti amvetsetse Mau Ake . — 1 Atesalonika 2 : 13 ; Yakobo 4 : 6 . Muli ndi thanzi labwino , mphamvu , ndiponso mulibe nkhawa . Mu 1958 , makolo anga anakwanitsa zimene anali kufuna . Iwo anagula nyumba kuti tonse atatu tizikhalamo . Baibo imakamba kuti panthawi ina , mtumwi Paulo pamodzi ndi anzake anavutika kwambili ndipo ngakhale miyoyo yawo inali paciwopsezo . Poona kuti sinikugonja pa cikhulupililo canga , asilikaliwo anayesa njila ina . ATSOGOLELI ACIPEMBEDZO nthawi zina amalosela zocitika zoopsa za padziko lapansi kuti acenjeze anthu ndi kusonkhanitsa otsatila ao . Wokwela pa hosi imeneyi akuimila njala . Imfa Ili Ngati Tulo Tofa Nato “ Walitsani maso anga kuti ndisagone mu imfa . ” — Salimo 13 : 3 . ‘ Anyamata ndi inunso anamwali , . . . tamandani dzina la Yehova . ’ — SAL . Tiphunzilapo ciani pa cikhulupililo colimba ca mayi ameneyu ? Masiku ano , abale athu ena ali m’ndende cifukwa ca cikhulupililo cao . Mwacitsanzo , Mose anauza Aisiraeli kuti apeleke zopeleka zothandizila pa nchito yomanga cihema . M’kupita kwa nthawi Ratana anasiya kutumikila Yehova , ndipo anayamba kupita ku cipembedzo cina n’colinga cofuna kukwatilana ndi mnyamatayo . ( Ŵelengani Deuteronomo 6 : 6 - 9 . ) “ Uwalamule kuti azicita zabwino , . . . kuti agwile mwamphamvu moyo weniweniwo . ” — 1 TIM . 6 : 1 - 27 . Mungakonzekele bwanji kuti mukakhale mtumiki wanthawi zonse ? 15 : 4 ) Sitiyenela kusintha maganizo popanda zifukwa zomveka . Ngati mucita zinthu monga zimenezi , acicepele adzayamba kudzimva kuti ali mbali ya “ mpingo waukulu . ” — Sal . Mwina mumasiyana ndi acinyamata ena monga mmene Mose analili wosiyana ndi acinyamata aciheberi ku Iguputo . 15 , 16 . ( a ) Kodi tikuphunzilapo ciani pa fanizo la Yesu la mwana wolowelela ? M’malomwake , anacilimika mwa kucita khama kupemphela . ( a ) M’fanizo la Yesu , kodi “ mlimi , ” “ mpesa , ” na “ nthambi ” zake ziimila ndani ? Pamene Paulo anali kufotokoza fanizo lake , mwina anali kuganizila zida zankhondo zimene asilikali aciroma anali kuvala . ( Mac . Ndiye ngati anthu amakwanitsa kutisoceletsa na mauthenga awo abodza , kuli bwanji Satana ? Iye ni “ mulungu wa nthawi ino . ” Eliya anamuuza kuti : “ Sikugwa mame kapena mvula zaka zikubwelazi , pokhapokha ine nditalamula . ” Sindinali kuyembekezela kuti amai anganene zimenezi . Ine na Janet tikupitiliza kutumikila pa ofesi ya nthambi ya ku Philippines mumzinda wa Quezon . Kupita patsogolo kwa zamankhwala kwathandiza ena kuthetsa kapena kucepetsa vuto lodwaladwala . Anati : “ Tinaonako tuzolengedwa tam’madzi twakufa tamakedzana ( ma ammonoids ndi ma trilobites ) . Lemba la Akolose 3 : 5 . ( Ŵelengani . ) limafotokoza zinthu zina zimene zingasokoneze ubwenzi wathu ndi Yehova . N’cifukwa ciani zinali zovuta kwa anthu ambili kukhala na Baibo m’nthawi ya John Wycliffe ? Makolo athu ndi Mboni za Yehova , ndipo akhala akuŵelengela Jairo nkhani za m’Baibulo kuyambila ali mwana . Mwina mukumbukila zitsanzo zina zoonetsa mapindu amene amabwela ngati Mboni za Yehova zipeleka ulemu woyenelela kwa olamulila a boma , mogwilizana ndi zimene Baibo imakamba . Imapeleka malangizo okhudza mbali zonse za umoyo wathu na mmene tingacitile tikakumana na vuto iliyonse . Ndiyeno , tinayamba kusakila nyumba . 1 : 4 , 11 ) Dalitso la Yehova linafika pamene Mfumu Aritasasita anasankha Nehemiya kukhala bwanamkubwa wa delalo . Timanyadila kutumikila Yehova motsogoleledwa ndi Mfumu yamphamvu imene Mulungu anaika . Pambuyo pake , wamasalimo anayamba kukamba za kumwamba . Iye anakamba kuti Yehova “ amawelenga nyenyezi zonse , ndipo zonsezo amazichula mayina ake . ” ( Sal . Onani kuti Marita anakamba kuti Lazaro adzakhalanso na moyo mtsogolo , “ m’tsiku lomaliza . ” Mokoma mtima , Gael anandipempha kukamwa tiyi kunyumba kwao . Komanso anali kuwelama kufika pa msinkhu wanga , na kukamba nane monga mabwenzi anga eni - eni . Izi n’zimene n’nali kufunikila kwambili pa nthawiyo . Mosasamala kanthu za kumene timakhala kapena ndalama zimene tili nazo , tonse tingagwidwe mu msampha wokonda cuma ndi kumangolakalaka kukhala ndi zinthu zambili zakuthupi kaya zinthuzo n’zofunika kwambili kwa ife kapena ayi , kaya n’zochipa kapena ayi . Iye afuna kuti abale amene azisamalila mpingo azikwanilitsa miyezo yapamwamba ya makhalidwe abwino . Timapemphelanso kwa Mulungu kuti , kupitila mwa angelo , atithandize kupeza anthu oona mtima . ( Mat . Ufumu Wa Mulungu — Ndi Boma Lopanda Ziphuphu 4 Kulalikila na kucezela mipingo kunan’thandiza kuphunzila kukamba Citagalogi . Komabe , tsiku lina atadzilimbitsa na kupezeka pa misonkhano , analemba kuti : “ Nkhani imene inakambiwa pa tsikulo inali yokhudza zinthu zimene zingatifooketse . Koma Nowa sanaonanepo ndi Inoki . 17 : 15 ) Molamulidwa ndi Yehova , Aisiraeli anamanga cihema . ( Eks . Ana amaona zimene mumacita ndipo zimawakhudza . Kodi Mulungu Wosaonekayo Mungamuone ? Anati : “ Uike Yoswa kukhala mtsogoleli ndipo umulimbikitse ndi kumulimbitsa , cifukwa ndiye adzawolotsa anthuwa ndi kuwacititsa kulandila dziko limene ulionelo kukhala colowa cawo . ” 3 : 16 , 17 ) Pamene tigwilitsila nchito mwaluso Mau a Mulungu ouzilidwa muutumiki , timapatsa ena mwai wodzalandila moyo wosatha . Koma cacikulu pa zonsezi ndi cikondi . ” — 1 Akor . Malinga ndi zocitika paumoyo , nthawi zina tingafunike kusintha maganizo athu ndi zocita zathu . N’cifukwa ciani Nadia amakondwela kuti sanacoke mumpingo wa citundu ca m’dziko limene anacokela ? Mnzanuyo atsegula citseko ndi kukuzani kuti muloŵe , ndipo mtima wanu ukhala pansi podziŵa kuti mwatetezeka tsopano . Ngati ndinu mkulu , muyenela kuŵelenga m’ndandanda wa ziyeneletso umenewu , ndipo ngati mwaona pamene muyenela kuongolela , muyenela kucita zimenezo mwamsanga . 2 , 3 . ( a ) N’cifukwa ciani Yehova ndiye woyenela kulemekezedwa koposa ? Kodi iye anaganiza kuti kucita mgwilizano ndi maufumu ena kapena kukhala na luso pa nkhondo n’kumene kukanam’teteza kuposa kudalila Mulungu ? Nditabwela kucokela ku Vietnam , ndinayamba kulakalaka kuphunzila za Mulungu . N’cifukwa ciani tiyenela kulalikila uthenga wa Ufumu kwa “ anthu osiyanasiyana ” ? Don na Margaret * anasangalala kwambili pamene mwana wawo wamkazi na banja lake anawacezela . Mkuluyo anali ndi colinga cabwino pamene anali kufunsa zimenezi . YELEKEZELANI kuti muyenda pamsewu usiku . 3 Anadzipeleka Mofunitsitsa — ku Russia Ndipo ndinaikidwa kukhala m’Komiti ya Nthambi . Nthawiyo , nthambi ya ku Austria inali kuyang’anila nchito ya m’maiko ambili a kum’maŵa kwa Europe . Ndipo inali kutumiza mabuku mwakabisila ku maiko amenewo . Ngati ndi conco , muyenela kukhala ndi cikhulupililo monga Eliya . MFUMU YAMUYAYA INALENGA ANGELO NDI ANTHU Koma ndinamuuza kuti : “ Ndine wokonzeka kufa , osati kumangidwa cabe . Poyamba iye anakamba ‘ mosazindikila . ’ Kodi Mulungu wacita ciani kuti tikhale paubwenzi wabwino ndi iye ? Tiyeni titengele citsanzo ca Yesu amene anati : “ Ndinatsika kucokela kumwamba kudzacita cifunilo ca iye amene anandituma , osati cifunilo canga . ” — Yohane 6 : 38 . KODI ndinu Mkhiristu ? Kulambila Mulungu ni mbali ya umoyo wathu , ndipo sitifunika kum’lambila mwamwambo cabe . Kudzilanga wekha kumaphatikizapo kudziletsa ku zinthu zina pofuna kuwongolela khalidwe lathu na maganizo athu . ( b ) Kodi mumamva bwanji mukaganizila cozizwitsa ca Yesu cimeneci ? 13 : 5 ) “ Cikhulupililo ” ndico ziphunzitso zonse zacikristu zopezeka m’Baibulo . Baibo imafotokoza kuti mmodzi wa zolengedwa zauzimu za Mulungu amene pambuyo pake anakhala wopanduka , Satana Mdyelekezi , anayesa kulepheletsa colinga ca Mulungu mu Edeni . Sitikukayikilani . ( a ) Kodi Paulo anauza Timoteyo kuti azisinkhasinkha za ciani ? Kodi kusinkhasinkha kumatanthauza ciani ? Ndipo tikambilana mafunso ati ? Ndipo n’cifukwa ciani ? Ganizilani za kusintha kumene kunapangidwa posacedwapa , monga kusintha kwa kaonekedwe ka zofalitsa zathu , nkhani zimene zimafalitsidwa , ndi kagaŵilidwe ka zofalitsazo . ( Aroma 10 : 2 , 3 ) Popeza analibe cidziŵitso ceni - ceni ca zimene Mulungu anali kufuna kuti io acite , cangu ndi cikhulupililo cao zinalibe phindu . — Mateyu 7 : 21 - 23 . Nthawi zambili a polisi anali kundikaikila cifukwa ca zocita zanga zacinyengo . Kodi timadalila nzelu zathu poyesa kuthetsa mavutowo ? Iye anali ndi uthenga wabwino wosatha woti aulengeze monga nkhani yosangalatsa kwa anthu okhala padziko lapansi , ndi kudziko lililonse , fuko lililonse , cinenelo ciliconse , ndi mtundu uliwonse . ( b ) Nanga Yehova anacitanji ndi zimene Satana anatsutsa mu Edeni ? Makhalidwe abwino ni ofunika m’nthawi ino imene zipangizo zamakono zili paliponse . Mphatso zina ni za mtengo wapatali cifukwa amene anatipatsa ni munthu waudindo , kapena ni munthu amene timalemekeza kwambili . Tiyenela kucita izi ngakhale kuti munthu amene tam’patsa moniyo sanaikileko nzelu . Ndithudi , Yehova amadziŵa zimene mtumiki wake aliyense angathe kucita . Kodi Yehova angakuthandizeni bwanji ngati mwacotsedwa nchito ? Komanso , ndiye anali kulandila magawo aŵili a coloŵa . — Gen . Cingalawa cinali umboni wosatsutsika wakuti Nowa anali munthu wodzipeleka pocita cifunilo ca Mulungu . Baibulo limatilimbikitsa kuti : ‘ Moyo wanu ukhale wosakonda ndalama , koma mukhale okhutila ndi zimene muli nazo pa nthawiyo . ▪ Kodi Cikumbumtima Canu n’Codalilika ? Mose analandila maphunzilo akuthupi apamwamba kwambili amene analipo panthawiyo . Koma kodi anawagwilitsila nchito kuti achuke mu Iguputo , adzipangile dzina , kapena kupeza cuma cakuthupi ? Onani mau awa a mneneli Mika : Hiroo ndi Svetlana ATAPITA KU KANANI Mkazi wake Sonja anavomeleza , ndipo anaonjezela kuti : “ Kukoma mtima n’kofunika kwambili . Zimakhala zosangalatsa kuceza ndi anthu a msinkhu wathu . Tikalandila udindo kapena utumiki wina wake m’gulu la Yehova , tifunika kuuona monga mwayi wathu woonetsa kuti tili na cikondi ceni - ceni mwa kupewa ‘ kudzifunila zopindulitsa ife tokha basi , koma zopindulitsanso ena . ’ Timacita cidwi ndi mmene amatipatsila cakudya cokonzedwa bwino ca kuuzimu nthawi zonse . ( Salimo 97 : 10 ) Ganizilani izi : Mukaona cinthu cimene cingaononge maso anu , mumacitapo kanthu mwamsanga kuti muwateteze cifukwa ndi amtengo wapatali kwa inu . Nayenso Yehova amacitapo kanthu mwamsanga kuti ateteze anthu ake cifukwa ndi a mtengo wapatali kwa iye . — Ŵelengani Zekariya 2 : 8 . Conco sitiloŵelela m’ndale za dziko ndi m’zocitika zina zocilikiza nkhondo . Kodi io acokela kuti ? Mwacitsanzo , anthu ena amaweluzidwa ndi kuikidwa m’ndende cifukwa cowanamizila kuti anapalamula mlandu winawake . 11 - 13 . ( a ) Ndani anagwilizana ndi anthu osankhidwa a Mulungu ? Abulahamu atakalamba , anapitilizabe kukhulupilila lonjezo la Mulungu ndipo “ cikhulupililo cakeco cinamulimbitsa . ” ( Mat . 24 : 14 ; Chiv . 22 : 17 ) Komabe , mabuku athu ena sapezeka m’zinenelo zina , ndipo anthu ena alibe kompyuta kapena intaneti kuti apeze mabuku athu . Nanga bwanji za amuna acikulile ? ZOKAMBA : Muzisankha mau abwino ( 2 Samueli 12 : 1 - 13 ) Davide anatipatsa citsanzo cabwino pankhani yodzicepetsa ndi kumvela . Ndangoitola cabe . ’ ( 1 Mafumu 21 : 29 ) Kodi Yehova anamukhululukila Ahabu ? Mosakaikila , otsatila a Kristu anali ndi nchito yopatsidwa ndi Mulungu . Iye anati : “ Tinadabwa titamva kuti tsiku lotsatila pambuyo pa civomezi , woyang’anila dela ndi m’bale wina anapita kwathu kukatifunafuna . ” Cakaco cisanafike , atumiki a Yehova anali kuona kuti khamu lalikulu ndi gulu la Akristu odzipeleka amene si acangu kwambili . 25 : 12 ) Cinanso , iwo analola anthu ena kuwasoceletsa , ngakhale kuwapangila zosankha . Baibo imatiuzanso kuti Mulungu anatipatsa mphatso kuti tikakhale na moyo wacimwemwe . Tiyeni tiziyesetsa kupezeka pamisonkhano yonse imeneyi kuti tikhale acimwemwe ndi olimba kuuzimu . — Tito 2 : 2 . Conco , tiyeni tipitilize kulola Yehova kutiumba , ndipo tizionetsa kuti timayamikila cilango cake cimene amatipatsa cifukwa cotikonda . — Miyambo 3 : 11 , 12 . N’cifukwa ciani tiyenela kukamba momveka bwino ? Kodi kuphunzila Mau a Mulungu kumatithandiza kudziŵa ciani ? ( Mat . 17 : 17 ) Conco , tisadabwe ngati ifenso nthawi zina tifunsa funso limeneli . Ndi khalidwe lotani limene atumiki a Yehova akhala nalo kuyambila kalekale ? Kukamba zoona , Yehova amatikonda monga ana ake , ndiye cifukwa cake amatipatsa cilango ndi kutiumba mwacikondi . Kodi oyenda panyanja akalekale anali kupanga bwanji ngalawa zao kuti madzi asaziloŵa ? — July - August Kodi Yehova na Yesu aonetsa bwanji kuti ni oleza mtima ? Anapitilizabe kutumikila monga mneneli kwa zaka 46 , mpaka mu ulamulilo wa Mfumu Hezekiya mu 732 B.C.E . N’ciani cinacitikila Solomo cifukwa conyalanyaza malangizo a Yehova ? N’cifukwa ciani tingakambe kuti n’zosatheka Yehova kucita zinthu mopanda cilungamo ? 14 : 3 . Conco , anali kuyelekezela kuti aone ngati ziphunzitso za chechi zinali zogwilizana ndi Mau a Mulungu . Kodi Yakobo anaonetsa bwanji kuti anali munthu wauzimu ? Atumiki okhulupilika a Mulungu m’nthawi ya Davide analinso odzicepetsa , okoma mtima , ndiponso olimba mtima . Tiyenela kukumbukila ciani ngati mantha amatilepheletsa kuimba mokweza ? 13 : 20 ) Mungacitenji kuti muteteze mwana wanu kuti zimenezi zisam’citikile ? Onsewa maina ao sadziŵika . Mwacionekele , tingaganize kuti wansembe waciisiraeli ndi Mlevi ndiwo anali anzake a munthu anamenyedwa uja ndi kusiidwa ali pafupi kufa . Coyamba , nchito ikulu panthawiyo inali kugaŵila mabuku ophunzilila Baibo . Kapepala kalikonse kali ndi lemba limene timaŵelenga ndi funso limene timafunsa mwininyumba . [ 1 ] ( ndime 1 ) Yesu anali kutanthauza boma pamene anakamba kuti Kaisara . Kuti tikhale oyela , tifunikila kuphunzila Malemba mosamalitsa ndi kucita zimene Mulungu amafuna . M’dela limodzi - modzilo , muli anthu acidwi amene timacitako maulendo obwelelako . ” Koma sindife tokha amene timaphindula . Yehova wakhala akuona mmene anthu akukhalila kucokela pamene anawalenga . Mwamuna wake anayamikila kwambili kuona mmene mpingo unatetezela mkazi wake na mwana wake . Cifukwa ca izi , anavomela kuphunzila Baibo ndipo anayamba kupezeka ku misonkhano pamodzi na mkazi wake ndi mwana wake . Tatyana anakhala kumeneko kwa nthawi yocepa ndi colinga cakuti apeze nchito imene idzamuthandize pocita upainiya . Kukonzekela Cikumbutso kungaphatikizepo kuganizila njila zina zoonjezela utumiki wathu . Mwina tingaciteko upainiya wothandiza pa nyengo ya Cikumbutso . Nthawi zambili filimu imeneyi anali kuionetsela panja , pa cinsalu cacikulu coyela cokoloŵeka pa nkhokwe . ( Miyambo 2 : 21 , 22 ) Anthu oipa sadzakhalaponso kuti acite zoipa . Mkulu wa opelekela cikho ndiye anayamba kufotokozela Yosefe loto lake . Ngati zingakhale conco , iye angakhale monga Akhristu a mu mpingo wa Aefeso wa m’nthawi ya atumwi . Ponena za Akhristu amenewo , Yesu anati : “ Wasiya cikondi cimene unali naco poyamba . ” ( Chiv . Komabe , palibe cifukwa comveka coti mwamuna kapena mkazi azilankhula mau onyoza ndi onyodola kwa mnzake , kapena kum’menya kumene . — Ŵelengani Miyambo 17 : 27 ; 31 : 26 . ( Zef . 3 : 8 , 9 ) Iye akutiphunzitsa kuti tizicita zinthu mogwilizana ndi colinga cake camuyaya . Kuyankha Mafunso a m’Baibulo Zoona zake n’zakuti , palibe pamene timaŵelenga kuti Davide anali wopemphapempha kuti apeze cakudya . Ameneyu anali munthu woyamba wochulidwa m’Baibo amene anaukitsidwapo . 27 : 9 . Koma atate anali kudana ndi cipembedzo ciliconse . M’maiko ena , mipingo imapanga makonzedwe akuti okalamba ndi odwala azimvetsela misonkhano pafoni . Mlengi wa anthu onse amatitsimikizila kuti “ akufa sadziŵa ciliconse . ” — Mlaliki 9 : 5 . ( b ) N’ciani cingatithandize kupitilizabe kuyenda panjila ya ku cipulumutso ? Yehova Mulungu anapanga makonzedwe ena oyenelela okhazikitsa mtundu watsopano . Apa , n’nali wokonzeka kupita . ” Akristu ena acinyamata mumakhala kumadela osauka , pamene ena mumakhala ku mizinda yotukuka . MASIKU ANO , anthu ambili amakonda kukamba za kukhala na ufulu . 10 : 12 ) Ngati tifuna kulimbitsa cikwati cathu , n’kofunika kukhalabe okhulupilika kwa Yehova ndi kwa mnzathu wa mu cikwati . Tingafunike kusiya zizolowezi zathu zimene zingatitaitse nthawi yocita zambili mu utumiki wa Yehova . ▪ Phunzitsani Ana Anu Acinyamata Kutumikila Yehova Anthu akhala akudzifunsa mafunso amenewa kwa zaka zambili . Tikamaona zocitikazo zikukwanilitsidwa timakhala otsimikiza kuti mapeto ali pafupi . Ise monga Akhristu , timakonda kwambili coonadi . Iye anati “ Ndinali kudziŵa zolinga zanga , koma kuzilemba kunandithandiza kuti ndiyesetse kuzikwanilitsa . ” Iye anapatsidwa uphungu mwacindunji ndi Mulungu , koma sanalabadile cifukwa ca kunyada . Ngakhale ndi conco , Mulungu adzacotsa zoipa zonse akadzabweletsa dziko latsopano , limene akufa onse adzakhalenso ndi moyo . — Machitidwe 24 : 15 . Pangano la mu Edeni ndiponso pangano la Abulahamu limatiphunzitsa kuti nthawi zonse ulamulilo wa Yehova ndi wozikidwa zolimba pa miyezo yake yolungama . ( Sal . 12 - 14 . ( a ) Kodi Danieli anaonetsa bwanji nzelu yaumulungu ? 33 : 24 ) Mukulakalaka kudzaonana ndi anthu amene adzaukitsidwa ndi kuyembekezela kukhala ndi moyo kwamuyaya . ( Yoh . Baibo imati : “ Iye wokhulupilila mwa Mwanayo ali nawo moyo wosatha . ” M’maiko ena , amuna amavutitsa akazi ao kapena kuwamenya pofuna kuonetsa kuti ndi olimba . Koma Baibulo limati : “ Munthu wosakwiya msanga ndi wabwino kuposa munthu wamphamvu , ndipo munthu wolamulila mtima wake amaposa munthu wogonjetsa mzinda . ” ( Miy . Kodi pali mphatso ina yamtengo wapatali kuposa imene ingapatse munthu moyo wosatha ? 3 Anadzipeleka na Mtima Wonse — Ku Myanmar N’ciani cingatithandize kuti tizimvela ena cifundo ? Kukhala okhwima mwauzimu kumaphatikizapo kuwonjezela cidziŵitso na luso lathu la kuzindikila . ( Genesis 12 : 17 - 20 ) Abulahamu anakondwela kwambili kukhalanso na mkazi wake wokondeka ! Alongo aŵili akulalikila uthenga wofunika kwa mwini shopu ku Montevideo , likulu la dziko la Uruguay Conco , iwo anauza Farao , ndipo iye analamula kuti mkaziyo amubweletse kwa iye . Yosimbidwa ndi Ronald J . N’cifukwa ciani Akristu onse oona akusangalala kudziŵa za cikwati ca pakati pa Kristu ndi mkwatibwi ? Si nthawi zonse pamene kucita zimenezi kungakupangitseni kukhala mabwenzi apamtima . Koma kungakuthandizeni kukhala ogwilizana ndi m’bale kapena mlongoyo . ( Sal . 1 : 1 - 3 ) Ndipo angalimbitsenso cikwati cao mwa kucita Kulambila kwa Pabanja kosangalatsa ndi kotsitsimula mwa kuuzimu . 1 : 1 ; 21 : 3 - 5 ) Ndani anauza Yohane kulemba mau amenewa ? Ndipo tingayambe kukaikila ngati Yehova amamva mapemphelo athu kapena ngati amationa monga mabwenzi ake . Mulungu wapeleka citsanzo cabwino kwa ise mwa kukwanilitsa malonjezo ake , ndipo ifenso amatithandiza kukwanilitsa malonjezo athu . 6 : 1 ) Kodi masiku ano tingaseŵenzetse bwanji malangizo a Paulo amenewa ? Kuyambila mu 1999 , nakhala na mwayi wotumikila m’Bungwe Lolamulila Mungacite ciani kuti mupalane ubwenzi wamuyaya na Mulungu ? ( Aef . 6 : 4 ) Mwacitsanzo , makolo angapemphe akulu kuti awauzeko zimene angacite pa kulambila kwa pabanja , ndi mmene angapezele mabwenzi abwino a ana awo . Mosiyana ndi Adamu , Yesu “ sanacite chimo . ” ( Salimo 104 : 5 ) Lemba limeneli ndi malemba ena amatitsimikizila kuti Mulungu sadzaononga dziko kapena kulola kuti lionongedwe . — Mlaliki 1 : 4 ; Yesaya 45 : 18 . Awa ni malo abwino amene Yehova watipatsa masiku ano otithandiza kuti tiumbike . N’cifukwa ciani zinakhala conco ? Dzina lakuti “ cinjoka ” limatipangitsa kuganiza za cilombo coopsa , ndipo ndi loyenelela Satana cifukwa amafunitsitsa kulepheletsa colinga ca Yehova ndi kuononga anthu Ake . Pa ana a Yakobo ( Isiraeli ) , woyamba kubadwa mwa Leya anali Rubeni . 3 : 1 , 2 ) Conco , ise monga Akhristu tifunika kucita khama kuti tizikonda kwambili Mulungu , coonadi , ndi anthu anzathu . Ndine wokondwa kuti Yaroslav na mkazi wake Alyona , ndiponso Pavel na mkazi wake Raya , akutumikila pa Beteli . Nayenso Vitaly na mkazi wake Svetlana akutumikila m’dela . Koma m’fanizo la matalente , Yesu anali kukamba za nthawi imene adzabwela kuŵelengela cuma cake ndi odzozedwa amene adzakhala akali padziko lapansi panthawi ya cisautso cacikulu . N’cifukwa ciani makolo acikhiristu ayenela kuonetsetsa kuti Mau a Mulungu akufika pamtima pa ana awo ? Komanso mphamvu yokwanitsa kuganizila zinthu zimene sitinazionepo imatithandiza kukhala ndi cikhulupililo . — 2 Akor . Masiku ano , timagwilitsila nchito makompyuta ndi Intaneti kulalikila anthu kulikonse , ngakhale m’madela ovuta kufikako . A Daka : Ndili bwino . Inenso ndasangalala . Poyankha iye anati , “ Sitingadziŵe , koma timangoganiza kuti mwina Mulungu Amawasamalila anthu amenewa . ” Iye anati : “ Mangani nyumba [ ku Babulo ] ndi kukhalamo . Kodi anthu ochulidwa pa Oweruza 5 : 9 , 10 anali osiyana bwanji ? Nanga ife tiphunzilapo ciani ? Komabe , aliyense wa ife ayenela kucitapo kanthu mosazengeleza kuti aleke kucita ciliconse cimene cingam’vulaze mwa kuuzimu . Mateyu 6 : 14 Ndaona kuti Yehova saiŵala kudzipeleka kwanga mu utumiki wanthawi zonse . Kuti tipeze yankho pa funso limeneli , coyamba tifunika kumvetsetsa tanthauzo la cimwemwe ceni - ceni , ndi mmene ena akhalilabe acimwemwe olo kuti amakumana na mavuto . Tiyenelanso kucita khama kuti tileke khalidwe lililonse loipa kapena cizoloŵezi ciliconse cimene cingatilepheletse kukaloŵa mu Ufumu wa Mulungu . ( Agal . Ndi masukulu ena ati amene tili nao ? Cilengezo cimene cinapelekedwa pa nthawiyo cinakamba kuti kusinthako kudzathandiza atumiki a pa Beteli kuti azikhala na mpata wocelezana pambuyo pa phunzilolo . 1 , 2 . ( a ) Kodi Solomo anauzilidwa kulemba uphungu wotani kwa acinyamata ? * — Mat . Conco , anayamba kukonzekela . Anacita zimenezo mwa kugwila nchito yolalikila Ufumu mwacangu . A Zulu : Mwayankha bwino . Cikondi ni khalidwe lalikulu la Mulungu . 19 : 18 . Kumalo ena , anthu ena anayenda mtunda wa makilomita 8 kuti akapenyelele “ Seŵelo la Eureka . ” Ni zilizonse zimene munthu angacite , zomwe mwauzimu n’zakufa , zopanda pake , komanso zosapindulitsa . 2 : 3 ) Nkhani ya kubadwa kwa Yesu inafala kwambili . Ndipo izi zinacititsa kuti ana ambili osalakwa aphedwe . — Mat . Ife tinathaŵila ku nyumba ya mkulu . 14 , 15 . ( a ) N’ciani cimene acicepele ayenela kukumbukila akayesedwa kuti acite zoipa ? Kodi komiti ya ciweluzo iyenela kuyesetsa kuzindikila ciani ? M’nkhaniyi tidzakambilana cifukwa cake nthawi zonse tifunika kucita khama kuti tikhalebe wodziŵika kwa Yehova , cifukwa kukhala wodziŵika kwa iye ndiye kofunika kwambili . Apanso zolemba zakale zinaonetsa kuti mau a m’Baibo ni oona . Abulahamu anacha mwanayo kuti Isaki , kapena kuti “ Kuseka , ” monga mmene Mulungu anakambila . Akhristu acatsopano amenewo anali ‘ kuvutitsidwa ndi anthu akwawo , ’ ndipo anafunika kulimbikitsiwa . ( 1 Ates . 2 : 14 ) Conco , ca m’ma 50 C.E . , Paulo analembela kalata mpingo wacatsopano wa ku Tesalonika . ( Gen . 2 : 18 ) Monga mmene Khiristu , mutu wa mpingo , amakondela kwambili mpingo wake , mwamuna wacikhiristu afunika kukhala mutu wacikondi . Mlongoyu anadabwa ndipo anakondwela kuti onse atatu anavomela kuphunzila Baibulo , ndi kuyamba kupezeka pa misonkhano ya mpingo . Odzozedwa okhulupilika amene amafa cisautso cacikulu cisanayambe , amakhala atadindidwa cidindo comaliza panthawi ya imfa yao . Atumiki amenewo anatsatila malangizo a Yesu . Koma kodi ife tikuphunzilapo ciani ? MFUMU MESIYA AYENGA NZIKA ZAKE ZOKHULUPILIKA N’ciani cimene tifunika kucita kuti tikapulumuke pamene dziko la Satanali lidzaonongedwa ? 3 Napeza Cimwemwe Cifukwa Copatsa Ngati pacitika zinthu zokuvutitsani maganizo , zokucititsani mantha kapena nkhawa , kambani naye Atate wanu wacikondi wakumwamba . Koma pambuyo pake n’nazindikila kuti cinacake cofunika kwambili kuposa nchito cinali kusoŵeka mu umoyo wanga . Mfumu Davide ndi munthu mmodzi wodziŵika bwino amene anacita chimo lalikulu . Nthawi zina , anali kundikhomela panja kapena kundimana zakudya . ( Sal . 19 : 7 - 9 ) Conco , zinthu zonse za m’cilengedwe zili ndi malo ake , ndipo zimagwila nchito mogwilizana ndi mmene Mulungu anafunila . Magazini imeneyo inakamba kuti anthu adzalekanitsidwa panthawi ya Ulamulilo wa Kristu wa Zaka 1000 , ndi kuti anthu amene anatengela khalidwe la Mulungu la cikondi pa zocita zao zonse adzachedwa nkhosa . Monga tinakambila m’nkhani yapita , ni Yehova yekha , Mlengi wa zinthu zonse , amene ali na ufulu wocita zilizonse — ufulu wopanda malile . Okalamba ndi mabanja ao ayenela kufufuza pasadakhale za thandizo limene lingapelekedwe . Kodi pali kugwilizana kwanji pakati pa kumvela na cikondi ? Ise anthu tili na zibadwa zosiyana - siyana . Zimenezi zimakometsa ubwenzi . 18 : 1 - 3 . Sinimacitanso mantha kapena kuda nkhawa na za kutsogolo . Nayenso Cecilia wa ku Philippines anakamba kuti : Monga kholo , ndimada nkhawa kwambili ndi ana anga komanso amai anga amene tsopano sakwanitsa kundidziŵa cifukwa ca ukalamba ndi matenda . ( 1 Mafumu 21 : 4 ) Pamene Yezebeli anaona kuti mwamuna wake ali ndi msunamo , mwamsanga anapanga ciwembu ca kupha Naboti ndi anthu osalakwa a m’banja lake n’colinga cakuti alande munda umene Ahabu anali kufuna . M’nthawi ya Akhristu oyambilila , cioneka kuti mtumwi Paulo ndi amene anacita zambili polimbikitsa Akhristu anzake . M’nkhani ino , tidzakambilana mafunso anayi okhudza zinthu zimene makolo ena acikhristu amada nazo nkhawa . Zinthu zimenezo n’zimene zimawalepheletsa kuthandiza ana awo kupita patsogolo mpaka kubatizika . “ Cotelo khalanibe maso cifukwa simukudziŵa tsiku kapena ola lake ” — MAT . ( 1 Akor . 7 : 16 ) M’mipingo yambili ya Mboni za Yehova , muli mabanja mmene Mkhiristu ndiye anathandiza ‘ kupulumutsa ’ mnzakeyo . 26 Magaleta na Cisoti Cacifumu Zimakutetezani N’zoona kuti tifunika kupeza ndalama zogulila zinthu zofunika mu umoyo , ndipo palibe vuto lililonse ngati munthu wasankha nchito imene amakonda . Nanga anali kugwila nchito yanji kuti azipeza zosoŵa za paumoyo wao ? N’cifukwa ciani nthawi zina Yehova angalole kuti tiyesedwe ? 20 , 21 . ( a ) Kodi mafumu anayi amene takambilana afanana m’mbali ziti ? Kupewa mtima wodzikonda kungatithandize kuika zofuna za ena patsogolo m’malo mwa zofuna zathu . ( Afil . TSAMBA 5 • NYIMBO : 5 , 84 Zimene Boazi anakamba zionetselatu kuti anadela nkhawa Rute podziŵa kuti anali mlendo . Pambuyo pokambilana nawo mfundo za m’malemba , anali kukhutila akadziŵa mmene Yehova amaonela zinthu . Ndiye cifukwa cake atangoukitsidwa , koma asanapite kumwamba , iye anapatsa ophunzila ake udindo waukulu . Poganiza kuti akaidi aja athawa , woyang’anila ndende anacita mantha cakuti anatenga lupanga kuti adziphe . Koma Paulo anafuula pomuletsa . Paulo , wozoloŵelana ndi maulendo a pamadzi , mosakaikila anali kudziŵa zimenezo . Koma Yehova amaseŵenzetsa ‘ dzanja lake lamanja lacilungamo ’ ndi kugwila ‘ dzanja lanu lamanja , ’ ngati kuti akukudonsani kuti mucoke pa malo oipa . Mwacitsanzo , Yesu anaphunzitsa khamu la anthu atakhala m’boti . Ngakhale n’conco , iye sanali kucita ndewo , koma ‘ analola kusautsidwa ’ monga mmene Baibo inakambila . ( Yes . Malangizo amene anapeleka pa mbali zimenezi ni ofunika ngako kwa ise masiku ano . Anapanga mgwilizano ndi mdani wa Mulungu , Mfumu yoipa Ahaziya , mwana wa Ahabu . Nthawi zonse nkhosa ndi mbuzi anali kuziŵeta ndi kuzidyetsela pamodzi nthawi ya masana . Kodi tifunika kucita ciani ngati ena akutipondeleza ? — Vesi 1 , na 2 . Koma Yehova amaticenjeza mosapita m’mbali . 17 , 18 . ( a ) Kodi colinga cacikulu cimene Yesu anali kucitila zozizwitsa cinali ciani ? Nayenso Atate wathu wakumwamba amatithandiza tikakumana ndi mavuto m’dziko loipali . Iye amatitetezanso kwa Satana amene ndi wolamulila wa dzikoli . Anthu amene ali na cikumbumtima cosaphunzitsidwa bwino ali monga sitima ya pamadzi imene ili na kampasi yosaseŵenza bwino . ( Aefeso 2 : 2 ) Pamene mtumwi Paulo anali mwana , anali kutsatila zocita za atsogoleli acipembedzo ca Ciyuda . Sara anaona kuti kuvutitsa kumeneku kunali kuika moyo wa mwana wake pa ciwopsezo . Kodi mudzasankha nchito yosafuna maphunzilo apamwamba ? “ Mulungu si Mulungu wacisokonezo , koma wamtendele . ” — 1 AKOR . Rosemary amene ali ndi ana atatu , anakamba kuti iye ndi mwamuna wake anali kuvomeleza akalakwitsa . 48 : 18 , 19 . Tinakondwela kwambili kukhala mu kilasi imodzi na Don Steele . Olo zinali conco , cifukwa cokonkha malangizo a m’Baibo , tinakwanitsa kuthetsa kusamvana na kuyamba kutumikila pamodzi mokondwela . Misece ingapangitse kuti vuto likule kwambili . cimatipindulitsa bwanji payekha - payekha ? ( Yohane 6 : 48 - 68 ) M’malo mwakuti aphunzile zowonjezeleka , iwo anakana kumvetsela zonse zimene Yesu anali kuwaphunzitsa . Koma tsopano anali atacoka . M’madzulo , pa tsiku lakuti maŵa adzaphedwa , Yesu anauza atumwi kuti : “ Ndikupatsani mtendele wanga . ” Patapita nthawi , ananipempha kusamukila ku Mpingo wa Buxton umene unali na ofalitsa ocepa ndipo unafunikila thandizo . Pa tsikulo , anthu pafupifupi 3,000 anabatizidwa , ndipo naonso analandila mzimu woyela . — Machitidwe 2 : 37 , 38 , 41 . Sanalole kuti zocita za ena zimufooketse . 13 : 4 ; Agal . 5 : 22 ) Kuleza mtima kumaphatikizapo makhalidwe enanso ofunika kwambili acikhristu . Koma si Akhristu onse panthawiyo amene anali kudziŵa zimenezi . Mwacitsanzo , Akhristu ena a ku Korinto anali kudzidalila . Banja lonse linali kusangalala kuceza naye cifukwa anali wansangala ndi wanthabwala . Mwacitsanzo , kodi akalandila udindo wowonjezela umenewo , adzakwanitsabe kusamalila zinthu zina zofunika ? Mwa kucita zimenezo , iye anaonetsa kuti ni wololela , wodzicepetsa , ndi wacifundo . Ndithandizeni . ” Anali Kukonda Anthu Cilamuloco cinali kukamba kuti munthu wodwala matendawo anali wodetsedwa . Tingatelo kuti mkaziyo anafunika kukhala kwa yekha cifukwa ca matenda ake . ( Lev . Ngakhale n’conco , abale ena amasankhabe kucotselatu ndevu zonse . ( 1 Akor . ( b ) Kodi kudziŵa Yehova kumatithandiza bwanji kuti tisamakaikile zocita zake ? Kumbukilani kuti pa tsiku la ubatizo wanu , munayankha kuti inde pamene munafunsiwa funso lakuti , “ Pamaziko a nsembe ya Yesu Khristu , kodi munalapa macimo anu ndi kudzipeleka kwa Yehova kuti mucite cifunilo cake ? ” Tinagwilana manja na kupemphela kuti , “ Yehova , conde , agaluwa akayamba kutiluma , tife mwamsanga cabe ! ” Zosankha zathu zingaonetsenso kuti timacilikiza ulamulilo wa Mulungu . A Inoki : Ohoo . Ndinamva ngati mmene mtumwi Paulo anamvelela . ( 2 Tim . 3 : 1 ) Conco , kuti tikhalebe maso kuuzimu tifunika kuika maganizo athu pa zinthu zakumwamba . ( 1 Ates . Onani , Mfumu yayamba kale kulamulila ndipo inu ndinu atumiki ake olengeza ufumuwo . Uthenga umenewu ni wofunika ngako , ndipo anthu onse afunika kuumva ! Pokhala makolo , tinazindikila kuti tinafunika kucita zinthu m’njila yakuti ana athu aziona kuti ndife ogwilizana . ( Salimo 83 : 18 ; 2 Akorinto 7 : 1 ) Conco , ngati munthu amayamikila ndi kulemekeza Yehova kwambili , amayesetsa kucita zimene angathe kuti am’kondweletse . Komabe , mfundo ya palembali mukhozanso kuiseŵenzetsa ngati mwasiyana maganizo na munthu wina . GWILITSILANI NCHITO BAIBULO KUTI MUKHALE NDI MAGANIZO OYENELA Tifunika kuonetsetsa kuti Mau a Mulungu atifika pamtima ndi kulimbitsa cikhulupililo cathu . ( Mateyu 26 : 38 ; Yohane 12 : 27 ) Iye anadziŵa kuti adzavutika kwambili mpaka kufa . Timamvela Mulungu mwa kupewa kukondela munthu wina wa ndale , kapena cipani ca ndale ciliconse ngakhale kuti cili ndi zolinga zabwino zimene zingatipindulitse . 3 : 1 ) Pamene akulu acikondi apeleka uphungu ndi malangizo osapita m’mbali ndi acikondi , mau ao ‘ angasangalatse m’mtima ’ wa m’bale . Kodi Yesu anathandiza bwanji Petulo pamodzi ndi ophunzila ena ? Anzanga onse amene n’nali kugwila nawo nchito yokolola pa dzuŵa angacitile umboni . . . kuti zimene nakamba n’zoona . Pambuyo pake , magaziniwa afalitsidwanso m’zinenelo zina . Iye anati : “ Mnyamatayo anali ndi mantha kwambili cakuti pamene anayamba kukamba nkhani , anayambanso kulila . ( Chiv . 21 : 8 ) Imfa yaciŵili imeneyi sidzaonongedwa cifukwa amene adzafa pa imfa imeneyi sadzakhalanso ndi moyo . ( Yohane 1 : 47 ) Yesu anali kudziŵa zimene zinali m’mitima mwa anthu . Iye anali wodzicepetsa . Kuganizila citsanzo ca Hezekiya kuyenela kutilimbikitsa kuleka ciliconse cimene cingasokoneze ubale wathu ndi Mulungu , kapena kutilepheletsa kuika zinthu zauzimu patsogolo . Nanga Mulungu analiyankha bwanji pempho la Asa ? ( Yohane 4 : 24 ; 17 : 17 ) Ndipo mtumwi Paulo anakamba kuti ngati tifuna kukapulumuka tiyenela ‘ kudziŵa coonadi molondola . ’ NYIMBO : 52 , 41 Mwamuna amene anam’funsila cikwati anam’lonjeza kuti sadzamuletsa kupita ku cipembedzo cake . 4 : 10 ; Yer . 1 : 6 ) Ngati na imwe mumamvela conco , kodi mungathetse bwanji vuto limeneli na kupitiliza kupita patsogolo ? BAIBULO limatiuza kuti “ Mulungu ndiye cikondi . ” Pakuti ndilibe wina wamtima ngati iye . ” — Afil . Isabella anakamba kuti : “ Sin’nali kufuna kuti Yehova azicita manyazi na nchito yanga , cabe cifukwa cakuti nimazengeleza . ” Izi sizitanthauza kuti onse anali olemela . ( Luka 20 : 34 - 36 ) , 8 / 15 Ganizilani Davide , mfumu ya Isiraeli amene tam’chula m’nkhani yoyamba ya nkhani zino . Zimenezi zingacititse ena mumpingo kukhumudwa ndi kusiya kutumikila Mulungu mwacimwemwe . Mulungu sanali kuona mwana wake woyamba kubadwa monga wopanda pake . ( Aroma 8 : 21 ) Izi zidzacitika cabe cifukwa ca kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova . Popeza Timoteyo anali ‘ kuitanila pa dzina la Yehova , ’ iye anafunika kucitapo kanthu kuti akanize zocita zosalungama za Akristu onyenga . Kodi Akristu anafunika kucita ciani mu 66 C.E ? Nanga anakwanitsa bwanji kucita zimenezo ? Nanga akulu mu mpingo angaonetse bwanji citsanzo cabwino ? ( Ŵelengani Danieli 12 : 4 . ) Angayambenso kudela nkhawa za tsogolo lathu . 16 : 14 , 16 ) Timakondwela kwambili pamene tithandiza anthu kudziŵa za cikondi ca Mulungu , ndi madalitso amene watilonjeza m’dziko latsopano . — Mat . ( 1 Maf . 21 : 1 - 16 ) Nsanja ya Mlonda yacingelezi ya mu 1932 , inafotokoza kuti Ahabu ndi Yezebeli anali kuimila Satana ndi gulu lake , ndi kuti Naboti anali kuimila Yesu , ndipo imfa yake inali kuimila kuphedwa kwa Yesu . Makolo ena ku Bermuda amati akakhala ndi nkhawa , amapemphela pamodzi ndi ana awo , kupempha citsogozo ca Yehova . Anthu amene amakonda Mulungu amadziŵa kuti kuba kwa mtundu uliwonse ‘ kumanyozetsa dzina la Mulungu [ wawo ] . ’ Pa khalidwe lililonse , tidzakambilana mafunso atatu otsatilawa : Kodi khalidwe ili limatanthauza ciani ? Baibo ifotokoza zimene tingacite kuti tikapulumuke Aramagedo . — Zefaniya 2 : 3 . Coipa kwambili kuposa pamenepo n’cakuti cikhulupililo cathu cingafooke , ndipo tingaleke kugwilizana ndi gulu la Yehova . Mwina angaope cifukwa cakuti analakwitsa zina zake m’mbuyomu , ndipo angaone kuti sangayenelele kutumikila monga mtumiki wothandiza kapena mkulu . Yehova anamva pemphelo lake ndipo anam’thandiza kuti apambane nkhondo . Mofananamo , Yehova angasankhe kusadziŵilatu zinthu zonse . NKHANI YA PACIKUTO | MUNGACITE CIANI KUTI MUZISANGALALA NDI NCHITO YANU ? 10 : 7 ) Koma citsanzo ca Solomo cikutiphunzitsanso zomwe zingacitikile munthu amene wanyalanyaza lamulo la Mulungu ndi kukwatila kapena kukwatiwa kwa munthu amene satumikila Yehova . — Mlal . Kodi nthawi zina acicepele angakhumbile ciani ? Nanga ni masitepu ati amene angathandize ? Kodi munacita maphunzilo otani kukoleji ? Anthu ambili safuna kuongoleledwa kapena kuuzidwa zocita . ( Yohane 17 : 3 ) Conco , n’zotheka kugonjetsa imfa . Imakambanso kuti Afilisiti anamanga msasa m’mbali mwa phili , pakati pa mizinda iŵili ya Soko ndi Azeka . Davide ananena kuti mlendo m’cihema ca Yehova “ sanena misece ndi lilime lake . . . ( Eks . 4 : 2 - 5 ) Cacinai , Yehova anasankha Aroni kukhala wolankhulilako Mose ndi kum’thandiza kukwanilitsa utumiki wake . ( Akol . 3 : 12 , 14 ) Cikondi codzimana monga ca Kristu cidzathandiza kwambili kuti banja likhale lolimba . 21 : 8 , 9 ) Kodi kuphunzitsa ena n’kofunika bwanji masiku ano ? ( 2 Timoteyo 3 : 15 ) Mwacitsanzo , Baibulo limati : “ Kumbukila Mlengi wako Wamkulu masiku a unyamata wako . ” Tili m’kilasi , M’bale Poetzinger nthawi zina anali kunifunsa coŵeleŵesa kuti , “ Mlongo Erika , kodi mau amenewa amatanthauza ciani m’Cijelemani ? ” Kodi zamoyo si zodabwitsa ? Satana poonetsa Yesu “ maufumu onse a dziko lapansi , ” ayenela kuti anaseŵenzetsa masomphenya , cifukwa kulibe phili lalitali limene munthu angakwelepo n’kuona maufumu onse a padziko . Atumiki ambili akale ndi amakono , adzimana zinthu zambili kuti atumikile Yehova mu utumiki wanthawi zonse . Ana anapitiliza kugwila nchito imene inamuthandiza kupilila cifukwa nchitoyo inali kumutangwanitsa kwambili . Komabe nchitoyo sinathetse cisoni cimene anali naco . Kuti tidzakhale na moyo wosatha tifunika kucita zimenezi . Anthu mumzindawo anali kulambila milungu yonama , ndipo ngakhale atate ake a Abulahamu anali kucita zimenezi . Zofalitsa zathu zingapeleke malangizo othandiza pa vuto limene tikulimbana nalo ndi mmene tingaligonjetsele . N’cifukwa ciani n’zovuta kudziŵa amene akulankhula m’Nyimbo ya Solomo ? Daniel na Miriam anali kuganiza kuti ndalama zimene anasunga zidzawathandiza potumikila m’dziko la Panama kwa miyezi pafupi - fupi 8 . Conco , khomo litatseguka lotumikila ku Wallkill monga anchito amene amayendela , anadziŵa kuti anafunika kusiya acibale ao ndi zinthu zimene amakonda . Mike , wa zaka 60 , ndi mkazi wake , Alice , atumikila ku zilumba za Pacific zaka zoposa 20 . Tikamagwila nchito imeneyi modzipeleka , timaonetsa kuti timakonda Yehova ndi Yesu . — Yoh . 14 : 15 ; 1 Yoh . 5 : 3 . Mneneli ameneyo pobwelela kwawo , anakumana ndi mkulu wina wacikalambile wa ku Beteli , mzinda wapafupi . Ziweluzo zake ndi zosasanthulika , ndipo ndani angatulukile njila zake ? ” — Aroma 11 : 33 . Komanso ndinu okondwa kugwilitsila nchito luso lanu cifukwa cakuti ciliconse cimene mukucita cikupindulitsa ena ndi kulemekeza Mulungu . Mukuyang’ana uku na uku kuti muone ngati mungapeze kamwala kena . Ndinalembedwa nchito ya usilikali ku Germany . Kuonetsa mzimu waubwenzi kungakuthandizeninso kuyambitsa makambilano mosavuta . Panthawi ya mapeto , Mwana wa munthu adzatumiza “ okololawo , ” amene ndi angelo , kudzalekanitsa tiligu wophiphilitsa ndi namsongole . Kodi abale acikulile afunika kuiona bwanji nkhani yosiyila acinyamata maudindo ? 19 : 17 ) Nafenso masiku ano , kukoma mtima kwathu kungathandize “ anthu kaya akhale a mtundu wotani ” kudziŵa coonadi ndi kuona mmene Yehova amawakondela . — 1 Tim . Mzimayiyo dzina lake anali Apun Mambetsadykova , ndipo anali wa Mboni za Yehova . Mai wina amene ali ndi ana aŵili aamuna ndipo ndi akhungu , anati : “ Kukamba n’kofunika kwambili kuti aphunzile zinthu . Pa ulaliki wake wa paphili , Yesu anafotokoza kuti cimwemwe ceniceni ndi citetezo sizimabwela cifukwa ca zinthu zakuthupi kapena mphamvu zathu . Muzikamba nawo mofatsa . Kwa nthawi yoyamba ndinadziŵa zimene iye anali kuganiza . Kudela lina lochedwa Nord - Pas - de - Calais anthu ambili a Cipolishi anakumana koyamba ndi Ophunzila Baibulo amene anali kulalikila mwakhama kumeneko kuyambila mu 1904 . Zinthu zosiyana - siyana zimene Yehova analenga n’zocititsa cidwi ndipo zimatipangitsa kusangalala ndi moyo m’njila zambili . Dzikolo linali lokongola monga munda wa Edeni . Koma munalibe akerubi oletsa anthu kuloŵamo . Kodi pakhala zotsatilapo zotani ? Kodi cikhulupililo cathu cingalimbikitsidwe bwanji ndi ( a ) mabwenzi abwino ? Iwo sakaikila zimenezi cifukwa ali ndi umboni wokwanila ndipo n’zimene tonsefe timakhulupilila . ZINTHU ZINA ZIMENE BAIBULO IMAKAMBA Mwacionekele , nchito yolalikila imene iye anagwila Cigumula cisanafike , inaphatikizapo kucenjeza anthu za ciwonongeko cimene cinali kubwela . Mmene Nowa anadziŵila Yehova . Iye anakula monga Mkatolika wolimbikila , ndipo acibale ake ena anali ansembe . Kodi taphunzila ciani pa maumboni atatu amene takambilana oonetsa kuti tikukhala m’masiku otsiliza ? Malamulo aciyuda anali akuti anthu amene aweluzidwa kuti aphedwe , akafa anafunika kuikidwa m’manda dzuŵa lisanaloŵe . Olo pali pano , anthu m’maiko ena amafalitsa nkhani zotinena , cifukwa cakuti timayesetsa kutsatila malamulo a Mulungu pa nkhani monga za cikwati na kugonana . Lembali limati : “ Yandikilani Mulungu , ndipo iyenso adzakuyandikilani . ” Mlongo Karen wa ku Canada , wa zaka za m’ma 70 , watumikila kwa zaka zoposa 20 ku West Africa . Lipoti lina linati “ anthu 805 miliyoni anali kudya mopeleŵela mu 2012 mpaka 2014 . ” ( Sal . 139 : 17 , 18 ) Tiyenela kuganizila zinthu zabwino zimene Yehova amaticitila cifukwa ca cikondi cake . Pokhala Akhristu , tifunika kudzipenda kuti tidziŵe mmene timaonela cuma ca m’dzikoli . Tingacite zimenezi mwa kudzifunsa mafunso monga awa : ‘ Ningaseŵenzetse bwanji cuma canga kuti nionetse kuti ndine wokhulupilika kwa Mulungu ? Adzakhala osafuna kugwilizana ndi anzawo , kapena kuti osafuna kukambilana kuti agwilizanenso na anthu amene anakangana nawo . Conco , muzilimbikitsa wofedwa osati cabe panthawi ya malilo pamene mabwenzi ndi acibululu ambili alipo , koma ngakhale kwa miyezi ingapo pambuyo pakuti ena abwelela ku zocita zawo za tsiku na tsiku . Kodi nkhaniyi imaonetsa kuti Sara anakamba maganizo ake mosonkhezeledwa na Yehova ? ( a ) Tiyenela kucita ciani kuti tikhale na umoyo wacimwemwe na wokhutilitsa ? Mfundo za m’Mau a Mulungu zimatilimbikitsa kupewa kuvala zothina , zoonetsa thupi , kapena zoutsa cilakolako . Oksana anati “ Titaona mapuyo tinazindikila kuti ku Russia kukufunikila alaliki a Ufumu kuposa ndi kale lonse . Olo kuti angelo ali na nzelu ndi mphamvu zapamwamba kwambili , pali zinthu zina zimene sadziŵa na zimene sangakwanitse kucita . — Mateyu 24 : 36 ; 1 Petulo 1 : 12 . Kutsogolo kwawo , M’bale Russell anaona sitima ziŵili zikulu - zikulu zapamadzi zimene zinali mkati momangidwa . Sitima yoyamba inali kuchedwa Titanic , ndipo inayo Olympic . Ngati tipitiliza kuŵelenga ndi kuphunzila Mau a Mulungu tsiku lililonse , cikondi cathu pa Yehova ndi Mau ake cimakula . Kukhala maso n’kofunika kwambili pamene tikuyesetsa kuonetsa kuwala kwathu . 5 : 15 , 16 ) Komabe , sitifunika kucita zimenezi na colinga cofuna cabe kutsiliza buku kapena kupeza mayankho oyankha pamisonkhano . Mwacitsanzo , sanawauze cabe kuti ayenela kufuna Ufumu coyamba ndi cilungamo ca Mulungu . 22 Muziika Maganizo Anu pa Nkhani Yaikulu 6 , 7 . ( a ) Kodi mau a Paulo amaonetsa bwanji kuti tifunika kucita khama kuti tivule umunthu wakale ? N’zoona kuti kupanga zosankha n’kovuta . Iyenso anali wa Mboni za Yehova . Ndi citsanzo cabwino citi cimene Yesu anapeleka kwa ife tonse ? Patapita zaka 5 , mkulu wanga anadzipha . ( Yesaya 50 : 4 ) Tiyenelanso kuganizila mmene mau athu angakhudzile ena . Mwamsanga anthuwo anasintha ndi kuyamba kuponya miyala Paulo cakuti anam’siya atakomoka . — Mac . Zimene Yesu anakamba kumapeto kwa fanizolo zingatithandize kudziŵa nthawi imeneyo . Patapita zaka zocepa , ine na atate tinayamba kupita pamodzi na amayi kumisonkhano . Ndipo acibale anga onse komanso anzanga anali kutumikila Yehova mokhulupilika . ( Gen . 22 : 10 - 13 ) Malo amene anapelekela nsembeyo anachedwa “ Yehova - yire . ” Kodi inuyo ‘ mumayang’anitsitsa pa pamphoto ’ imene mudzalandila ? Anakankha njinga yake pa mtunda wa makilomita 320 kudutsa m’madela amene anthu ena kumbuyoku anafa cifukwa ca ludzu . Conco , Akhristu okwatilana ali na ufulu wosankha kuseŵenzetsa njila zina za cilezi ngati safuna kukhala ndi ana ambili , kapena ngati safuna kukhala ndi ana pali pano . Kodi cikondi ca Yehova cimatanthauzanji kwa imwe ? Ngakhale kuti tingakhale na ndalama kapena zinthu zocepa , zinthu zimene tingawacitile mokoma mtima zingawaonetse kuti Yehova amawakonda . Ngati mai kapena mwana wake wamwalila cifukwa covulazidwa , oweluza amodzimodzi anali kulamula kuti munthu wolakwayo aphedwe . Pambuyo pake , Akhiristu atsopano amenewa “ anapitiliza kulabadila zimene atumwiwo anali kuphunzitsa . ” ( Machitidwe 14 : 17 ; 17 : 26 - 28 ) Ngati tiphunzila Mau ake Baibo , tidzam’dziŵa bwino Atate wathu wakumwamba . Iye anacotsa mbusa amene anali pa udindowo ndi kumuuza kuti : “ Sindifunanso kuti uziphunzitsa Mau a Mulungu muno popeza unamangidwa cifukwa ca kuba za m’chalichi ! ” 2 : 2 ) Tate wobatizika sayenela kuganiza kuti , ‘ M’cikhalidwe ca kwathu kuphunzitsa ana ni nchito ya mkazi . ’ Pa gilasi ya patsogolo panali mau akuti “ Tengani motoka yanu . Nakubwezelani monga mphatso . Monga Akristu oyambilila , nafenso tingaonetse kuti timakonda Yesu potsatila malangizo ake pa nkhani ya pemphelo . Olo pamene n’nakula , nthawi zina n’nali kupitiliza kuganizila zimene wina wanilakwila kwa masiku angapo , kucita kusoŵa tulo , ” anakamba conco mayi wina dzina lake Patricia . ( Luka 4 : 43 ) M’mau ake otsiliza asanabwelele kumwamba , Yesu analangiza ophunzila ake kukhala mboni zake mpaka “ kumalekezelo a dziko lapansi . ” Ndiye cifukwa cake timadwala , timakalamba , ndi kufa . Kodi tili na mipata iti yoceleza ena ? Kodi cimacitika n’ciani munthu akamwalila ? ( Mac . 14 : 3 ) N’cifukwa ciani timalalikila molimba mtima ? Aisiraeli anayamba kuona ngati kuti ali okha - okha m’cipululumo popanda mtsogoleli aliyense . ( Luka 21 : 2 - 4 ) Abale ndi alongo amayamikila citsanzo cabwino ca kukhulupilika ndi kupilila cimene abale ndi alongo acikulile amasonyeza . 90 : 10 ) Ena amaganiza kuti maboma a anthu adzathetsa mavuto . Koma Baibulo limaonetsa kuti Ufumu wa Mulungu wokha ndi umene udzathetsa mavuto onse a anthu . ( Dan . Zimene ofalitsa nkhani amakamba . ya July 2009 , muli mfundo yakuti ngati mnzanu wotsutsa ku sukulu wakufunsani kuti : “ N’cifukwa ciani sukhulupilila cisanduliko ? ” Iye anazindikila kuti zimenezi sizinacititse mwana wake kuyamba kum’konda . Kuwonjezela apo , mu 2015 Bungwe Lolamulila linafalitsa kabuku kakuti Bwelelani kwa Yehova . Kabuku kameneka kakhala kolimbikitsa kwambili kwa abale na alongo oculuka pa dziko lonse . Anthu amenewa anasonkhana m’cipinda capamwamba ku Yerusalemu . ( Mac . Udzaloŵa m’malo ulamulilo uliwonse wa anthu . Pa nthawi ina , bungwe lolamulila linapemphedwa kuti ligamule ngati kunali koyenela kuti Akhristu a mitundu ina azicita mdulidwe , monga mmene Ayuda anali kucitila potsatila Cilamulo ca Mose . Pofuna kutsimikizila ulosi umenewu , vesi 5 limati : “ Mau awa ndi odalilika ndi oona . ” Koma ine ndimakhulupilila kuti Baibulo ndi lothandiza masiku ano . Ambili athandizidwa cifukwa cophunzila bulosha lacingelezi lakuti , The Origin of Life ​ — Five Questions Worth Asking , ndi buku lakuti Is There a Creator Who Cares About You ? Baibo imakamba kuti Paulo anali ‘ kutanganidwa kwambili ndi nchito yolalikila Mau a Mulungu . ’ ( a ) Fotokozani citsanzo coonetsa ngozi imene ingakhalepo ngati timakonda kwambili zosangulutsa . ( b ) N’ciani cingatithandize kuti tiziona zosangulutsa moyenela ? Koma ndani kwenikweni amene amaika abale pa udindo ? Vuto laciŵili linali lakuti , Kingsley anali kuŵelenga movutikila ndi kugwila zinthu zocepa kwambili . Kodi akulu ayenela kuiona bwanji nchito yophunzitsa ena ? Mu 1966 , ofesi ya nthambi ya ku Dublin inayamba kuyang’anila cigawo ca kumpoto ndi ca kum’mwela kwa Ireland . Izi zinacititsa kuti abale na alongo akhale ogwilizana kwambili . Conco , iwo anaona kuti Yesu akanakhalapo , sembe mlongosi wawo Lazaro sanamwalile . Timakondwela tikamamva kamphepo kayeziyezi , tikamaothela dzuŵa , tikamadya cipatso cokoma kapena tikamamvetsela kuimba kotsitsimula kwa mbalame . Iye anawauza kuti : “ Yehova Mulungu wako adzakucititsa kukhala ndi zinthu zosefukila pa nchito iliyonse ya manja ako . ” ( Deut . Tikamaona mmene Yehova amatikondela , timayamba kum’konda kwambili . Iye anaona mmene Yehova anawadalitsila kaamba ka mzimu wodzipeleka umene anali nao moti anakamba kuti , ‘ Inenso ndifuna ndikacite zofanana ndi zimenezo . ’ Tinalinso kulalikila m’sitima popita ku Balykchy na pobwela . Mulungu amaonetsa cikondi cake m’njila zambili osati cabe kutisamalila mwakuthupi . Nkhani zotsatila zidzafotokoza mbali zitatu zimenezi . 12 : 15 . 15 , 16 . ( a ) Fotokozani mmene mlongo wina analeledwela . ( b ) Nanga n’cifukwa ciani iye sanafune kupatsa amai ake udindo wolela mwana wake ? Dziko limene lomba limachedwa Kyrgyzstan linali pansi pa ulamulilo wa Soviet Union . A Mboni za Yehova ni okonzeka kukuthandizani . Sindinali kudziŵa kuti nthawi imeneyo moyo wanga udzasinthilatu . ( Aroma 8 : 20 , 21 ; Chiv . ( Eks . 5 : 2 , 6 - 9 ) Apa umboni unali woonekelatu kuti Yehova anali atasankha Mose kukhala mtsogoleli wa anthu Ake . Komanso , mogwilizana ndi zimene Lije anakamba , “ makolo ambili amene anaona acibale awo akugwililidwa ndi kuphedwa , sangalole kuti iwo ndi ana awo abwelele kumalo kumene zoipazi zinacitikila . ” ( Yobu 16 : 1 - 5 ) Pambuyo pake , Yobu analandila cilimbikitso kucokela kwa Elihu , komanso analimbikitsidwa mwacindunji na Yehova . — Yobu 33 : 24 , 25 ; 36 : 1 , 11 ; 42 : 7 , 10 Koma mwina mungafunse kuti , ‘ Ndani anagaŵa Baibulo kuti likhale m’macaputala ndi m’mavesi ? ’ Vuto la ziphuphu za m’boma n’lovuta kwambili kuthetsa . Angelo ni zolengedwa zauzimu zapamwamba kwambili , zanzelu , ndi zamphamvu . ( 1 Yohane 4 : 9 , 10 ) Yesu anauza otsatila ake kuti azikumbukila imfa yake pa mwambo wosavuta mwa kugwilitsila nchito mkate ndi vinyo . N’nali kucita izi kaŵili kapena katatu pa wiki . ” Kucita zimenezi kunali kum’thandiza kucepetsako nkhawa . Yehova samangouza ife anthu kuti tikhale oleza mtima , koma iyeyo watipatsa citsanzo cabwino kwambili pa nkhani imeneyi . 14 : 4 ) Sara anaganiza kuti anali ‘ wothelatu ’ cifukwa ca ukalamba . ( Gen . Nkhondo Imene Inasintha Zinthu Padziko ( Nkhondo yoyamba ya padziko lonse ) , 2 / 1 Tingadzifunse kuti : ‘ Kodi ana anga adzakhala ndi tsogolo labwino ? Kodi Yesu anapeleka fanizo lotani pofuna kuticenjeza kuti ‘ tisamade nkhawa za tsiku lotsatila ’ ? Kukula kwake kumayamba kuonekela pakapita nthawi . ( a ) Kodi Yehova anawauza ciani Aisiraeli atangotuluka mu Iguputo ? ( Eks . 11 : 4 - 8 ) Ndiyeno , anauza mabanja aciisiraeli kupha mbuzi kapena nkhosa ndi kuwaza magazi pamakomo a nyumba zao . Nyama imeneyi inali yopatulika kwa mulungu wa Aiguputo wochedwa Ra . ( Eks . Tingacite ciani kuti tisagonje ku zilakolako zoipa ? 1 : 7 ) Pa 18 December , 1974 , tinavomelezedwa mwalamulo kuti tizilambila mwaufulu . ( Yohane 11 : 43 ) Womwalilayo anatuluka , ndipo anthu amene anali kuonelela anadabwa kwambili . ( Aroma 15 : 4 ) Citsanzo ca Abulahamu , Sara , Isaki , Yakobo , Mose , Rahabi , Gidiyoni , Baraki , ndi ena ambili cingatithandize kulimbitsa cikhulupililo cathu . Pa anthu amene analemba Baibulo , ndi mtumwi Yohane cabe amene anachula mau akuti “ wokana Kristu . ” N’zoona kuti nthawi zina tingafunse kuti : “ Mpaka liti , Yehova ? ” Baibo imati : “ Anthu amene amaopa Mulungu woona zidzawayendela bwino . . . , Koma woipayo sizidzamuyendela bwino n’komwe , ndiponso sadzaculukitsa masiku ake . ” ( Mlal . Pamene tikuyandikila ku mapeto kwa “ masiku otsiliza , ” makhalidwe a anthu ena amene timawalalikila “ adzaipilaipilabe . ” ( 2 Tim . Tifunikanso kupemphelela abale athu padziko lonse , makamaka “ amene akutsogolela pakati [ pathu ] . ” Utali wa phunzilo limeneli ukudalila zimene inuyo mufuna kuphunzila . Nanga bwanji za mavuto amene anazika kale mizu , ndipo aoneka kuti sadzatha ? Anthu ena amakhulupilila kuti umoyo wawo unakonzedwelatu ndipo sangausinthe . ( 2 Mbiri 16 : 9 ) Conco , tingakhale ndi cidalilo cakuti zimene timacitila Yehova ‘ mocokela mumtima ’ sizidzapita pacabe . — 1 Tim . Anthu a m’maiko osiyanasiyana ndiponso a zikhalidwe zosiyanasiyana anali kukonda M’bale Pierce cifukwa cakuti anali wansangala ndipo anali kukonda kumwetulila . Mwacitsanzo , tiyelekezele kuti imwe muli na vuto losoŵa tulo . Koma amafunanso kuti tisamadzione kukhala apamwamba kwambili kuposa ena . — Aroma 10 : 12 . Mkati mwa kuceza kwawo , wofalitsa angaloŵetsepo mfundo ya palemba , na kum’funsapo funso . Aonetsanso kuti Ufumu wa mtendele uli pafupi . ( 2 Mbiri 16 : 1 - 3 ) Pamene Basa anaukila Yuda , Asa anadalila nzelu zake ndipo anatumiza cuma kwa Mfumu Beni - hadadi ya Siriya kuti ikalimbane ndi Basa . ( b ) Nanga n’ciani cidzacitikila omwe adzakhala ngati anamwali opusa ? Popeza n’nali mmodzi wa anthu oyendetsa boti , ananilola kukhala m’dzikolo mwezi umodzi cabe . M’ndime zotsatila , onani nkhani , mafunso , ndi malemba amene mungagwilitsile nchito m’gawo lanu . * ( Gen . 42 : 1 , 2 ) Masiku ano , anthu ambili amapita ku maiko ena osati cifukwa cakuti mabanja ao akusoŵa cakudya , koma kukafunafuna ndalama kuti abwezele nkhongole zazikulu , ndipo ena amangofuna kulemela . M’pomveka kuti nthawi zina munthu amasoŵa cokamba kwa munthu amene ali na cisoni cacikulu . Kupanga ophunzila ni nchito ya gulu osati ya munthu mmodzi . Kodi Yesu anavomela pempho lake ? Mouzilidwa , mtumwi Paulo anafotokoza zimene Akhristu a ku Korinto anacita atalapa . Amadziŵa kuti anthu ni opanda ungwilo ndipo amamvetsetsa zofooka zathu , “ amakumbukila kuti ndife fumbi . ” — Salimo 103 : 8 , 9 , 14 . 16 : 5 - 10 ) Komabe , sikuti nthawi zonse Davide anali kudziletsa . Panthawiyo , ku nyumba zogona alendo sanali kusamalila bwino alendo , ndiponso kunali kucimake kwa khalidwe loipa laciwelewele . Koma imaticenjeza kuti tifunika kupewa kumwa kwambili ndi ucakolwa . ( Miy . 20 : 1 ; 1 Tim . ( Mal . 3 : 7 ) Mfundo imeneyi ikugogomezeledwa m’fanizo lina limene Yesu anafotokoza la mwana woloŵelela . — Ŵelengani Luka 15 : 11 - 32 . Malinga n’zimene linakamba buku lakuti Journal of Happiness Studies , munthu amakhala wacimwemwe akakhala na zinthu zofunikila kweni - kweni mu umoyo , monga cakudya , vovala na pogona . Yesu ali pafupi kuukitsa bwenzi lake Lazaro , anati : “ Ine ndine kuuka ndi moyo . ” Mobwelezabweleza ndinafuna kusonkhanitsa ana ako pamodzi , muja nkhuku yathadzi imasonkhanitsila anapiye ake m’mapiko . Kodi anthu amene atumikila mumpingo wa cinenelo cina angacite ciani kuti akhalebe auzimu ? Monga mmene Yesu analonjezela , iye ali nafe kuti atithandize . ( Mat . Pofotokoza zotulukapo zake , iye anati : “ N’nacotsa mimba katatu . ” ( Yohane 3 : 3 - 6 ) Cimene Yesu anali kulonjeza wocita zoipayo n’cakuti adzakhalanso ndi moyo , m’Paladaiso . Kupeleka zopeleka zocilikiza nchito ya Ufumu ndi cosankha cathu . Petulo anali mmodzi wa anthu amene anali kutsogolela mu mpingo woyambilila wacikhristu . Kumbukilani kuti ngati anzanu ali ndi imelo adilesi , naonso amagwilitsila nchito Intaneti ndipo akhoza kufufuza zinthu zimene zingawakondweletse , m’malo moyembekezela inu . Iye amakonda kwambili ulaliki , ndipo sindinali kufunika kumulimbikitsa kupita mu ulaliki . Conco , ‘ tingamuyang’anitsitse ’ bwanji Yesu ? Koma pamene Paulo ananena kuti iwo anali “ ngati akufa ku ucimo , ” anali akali na moyo , ndipo anali kutumikilabe Mulungu padziko lapansi . ” ( Deuteronomo 19 : 15 ) Cilamulo ca Mulungu cinalamula mboni kuti : “ Usafalitse nkhani yabodza . ( Mateyu 7 : 9 - 11 ) Zoonadi , Mulungu akukupemphani kupemphela kwa iye cifukwa “ amakudelani nkhawa ” ndipo amafuna kukuthandizani . ( 1 Maf . 3 : 23 - 27 ) Komanso kumbukilani za mwana wamkazi wa Farao , amene anapulumutsa Mose pamene anali wakhanda . ( Genesis 11 : 30 ) Malinga ndi cikhalidwe ca m’nthawi imeneyo , limeneli linali vuto lalikulu . Pamene tinabwelela ku Australia , tinadabwa kudziŵa kuti taitanidwa kukatumikila monga amishonale mumzinda wa Funafuti pacilumba ca Tuvalu , kumene kale kunali kuchedwa zilumba za Ellice . Ndi cosankha canzelu citi cimene acinyamata acikristu ayenela kupanga ? Ninawauza kuti sitidzapita kuti tizithandiza mlongosi wanga Linda kuwasamalila . Anthu ambili aona kuti Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika ni lolongosoka , lodalilika , ndi losavuta kumva . Anakamba kuti : “ Umishonale waniphunzitsa kukhala wodzimana , wacikondi ndi woleza mtima . Mabuku anu amafotokoza zinthu mosiyana ndi mmene timakambila m’cinenelo cathu . ” Mofananamo , Mfumu yathu yatipatsa zida zimene tingagwilitsile nchito kuti tithandize anthu kulandila uthenga wathu . Yesu sanamuuze kuti abwelele iyayi , koma anapatula nthawi kuti amuphunzitse coonadi ca mtengo wapatali . ( Yoh . ( b ) Kodi tiyenela kupewa kakambidwe kotani ? “ Wodala ndi munthu amene amaŵelengela ena mokweza , ndiponso anthu amene akumva mau a ulosi umenewu . ” — Chivumbulutso 1 : 3 . ( 1 Akorinto 9 : 16 ) Ngati titengela Paulo , tidzakhala ndi cikumbumtima cabwino , podziŵa kuti ticita zabwino . VUTO LIMENE LINALIPO : Abusa ndi atsogoleli a ndale ambili anali ndi zolinga zosagwilizana ndi uthenga wa m’Baibulo . Komabe , sitinaleke kutumikila Mulungu wathu wokhulupilika . ( Chiv . 5 : 9 , 10 ; 7 : 4 ) Pangano limeneli limawalola kulamulila ndi Yesu kumwamba . Ni zinthu ziti zimene tiyenela kuganizila popenda uzimu wathu ? Adolfo anati : “ Kupemphela kwa Yehova nthawi zonse kwanithandiza kwambili , maka - maka pamene zinthu sizinali bwino . ” Kodi anafunika kulowabe mkati kukapenyelela vidiyoyo ? Ndimupangila womuthandiza , monga mnzake womuyenelela . ’ ” — GEN . Ndipo kukhala oona mtima kumatithandiza kukhala ndi cikumbumtima coyela , cimene n’cinthu ca mtengo watapali . Koma pamene anthu m’dela lake anayamba kucita ciwawa cifukwa cosiyana mitundu , maganizo a tsankho anayambanso kukula mumtima mwake . Ngakhale n’telo , io anapitabe kunkhondo cifukwa ca cilimbikitso ca mkaziyu . Mlongoyo anangokhala pampando osayankha . ▪ “ Munavomeleza Kuti Zimenezi Zicitike ” ( Aheb . 2 : 14 ) Sikuti iye amapha anthu mwacindunji . “ Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi ? ” Mkazi wina anati : “ Mwamuna wanga atakhumudwa , analeka kundikambitsa kwa masiku angapo . Anne anauza amai ake kuti angakhalenso osangalala kokha ngati abwelela kwa Yehova . — Yakobo 4 : 8 . Nanga n’cifukwa ciani Yesu anakamba kuti sitiyenela kudela nkhawa zinthu zimenezi ? Nanga n’cifukwa ciani tifunika kuigwilitsila nchito mosamala ? Izi zinathandiza kuti mayiyo akwanitse kubweza nkhongole yake , na kutsala na ndalama zina zokwanila kusamalila banja lake . Tili ndi umboni wodalilika wa anthu amene anaona ndi maso zimenezi . ” — Ŵelengani 1 Akorinto 15 : 3 - 8 . ( Afil . 2 : 9 - 11 ) Ngakhale kuti Yesu anali ndi udindo waukulu , modzicepetsa anagonjela kwa Atate wake . Ambili a ise tasintha zinthu zambili pa umoyo wathu kuti tikhale nzika za Ufumu wa Mulungu . Coyamba , Yaeli anafunika kuganiza cocita mwamsanga . Mphunzitsi wina wophunzitsa za mavinidwe anakhazikitsa kampani ya zovinavina mumzinda wa Wuppertal , ku Germany . Iye anasankha ine ndi Gwen kuti tikhale m’gulu lake la ovina . Tidzakhala osangalala kwambili pamene tidzatumikila Yehova kwamuyaya pamodzi ndi anthu amene timakonda ! N’ciani cingakuthandizeni ngati mumaopa kuuzako ena zikhulupililo zanu ? Kulikonse kumene ndinali kupita , ndinali kukhala ndi mfuti yanga ( A . N’nakwela mpaka kufika mamita 8 . ( Salimo 15 : 1 - 5 ) Conco , ngati tifuna kuyandikila Mulungu , tiyenela kuyesetsa kutengela iye ndi Mwana wake . Anthu ena akandikhumudwitsa , ndimayesetsa kusakwiya msanga ndipo nthawi zina ndimangocokapo . Milungu ya anthu a mitundu ina inalephela kupeleka umboni woonetsa kuti ndi yoona . ( Agal . 2 : 11 - 14 ) Pambuyo podzudzulidwa , Petulo sanasunge cakukhosi kapena kuona kuti dzina lake laipa cifukwa ca uphungu wa Paulo . Kuwonjezela apo , pali zinthu zina zimene zimakhudza mtima wa mwana kupatulapo citundu . Kuuka kwa Yesu kumatsimikizila kuti zimene anaphunzitsa n’zoona . Kukamba zoona , n’zosatheka makolo kutsatila ndendende citsanzo cabwino kwambili ca Mulungu ca kudziletsa . Shane , amene tamuchula m’nkhani yapita , anati : “ Atate anga ndi munthu wolimbikila nchito kwambili . Ndipo tikamagwilitsila nchito zinthu zamakono monga webusaiti yathu ya jw.org pofalitsa coonadi , timasonyeza kuti tikutsanzila Yehova amene amafunitsitsa kupeleka malangizo othandiza kwa munthu aliyense . Thandizani Ena Kupita Patsogolo , 6 / 1 Nilongoze ! ” 17 : 15 , 16 ; 18 : 36 ) Cinanso , tidziŵa kuti Satana amafuna kuipitsa mbili ya Yehova na kuiŵalitsa anthu dzina lake . ( Mateyu 24 : 21 , 22 ) Ndipo Mulungu amatilonjeza kuti ambili adzapulumuka . Baibulo limati : “ Dziko likupita . . . , koma wocita cifunilo ca Mulungu adzakhala kosatha . ” — 1 Yohane 2 : 17 . Enanso samvetsela cifukwa cakuti anauzidwa mabodza ponena za zikhulupililo zathu . Onani cithunzi m’maganizo mwanu ca cimwemwe cimene mudzakhala naco podzawaonanso acibale anu amene anamwalila kalekale ndi podzawaphunzitsa zimene Mulungu adzakhala atawacitila . Ngati zinthu zofanana ndi zimenezi zakucitikilani , kodi mumatha kuzindikila cifunilo ca Yehova ? — Aefeso 5 : 17 . Pamene anali pa dziko lapansi , Yesu anakamba kuti anali kulakalaka kukhalanso na ulemelelo umene anali nawo poyamba , pamene anali ndi Atate wake kumwamba . ( Yoh . 2 : 3 . Cikhulupililo ca Sara cinam’cititsa kusiya umoyo wabwino kwawo Amayi ake a Nadia , a Marie - Madeleine , amene anali kukhala ku France , anagwa ndipo anathyoka dzanja na kuvulala ku mutu . Tsopano , tiyeni tione mmene Yehova analimbikitsila anthu ake kupitila m’masomphenya a Zekariya a namba 6 na 7 . Kodi zimene Boazi anacitila Rute mkazi wacimoabu , zionetsa bwanji mmene Yehova amaonela alendo ? Coyamba , Yehova amatiuza za iye cifukwa amafuna kuti timudziŵe . Makolo acikhristu amaona moyo wauzimu wa ana awo kukhala wofunika ngako kuposa zofuna zawo . ( 1 Akor . Munthu waciŵili wochulidwa m’Malemba amene anaukitsidwa , anamuukitsa ni mneneli Elisa , amene analoŵa m’malo mwa Eliya . Mwacitsanzo , amacita zinthu moganizila ena . — w17.10 , peji 7 . Ng’ombe zowondazo zinayamba kudya zonenepa zija . Pambuyo pake , Farao analota loto lina . Mungalipeze pa www.jw.org Zimenezi zingatheke tikamaphunzila mwakhama Mau a Mulungu ndi kuwasinkhasinkha . ( Sal . 6 : 4 , 6 . Limbani Mtima Yehova ndi Mthandizi Wanu , 4 / 1 Ni mafunso anji amene tingakhale nawo pa nkhani ya kuuka kwa akufa ? Kodi Mulungu amafunafuna bwanji munthu wosocelayo ? Nthawi imeneyo , mkaidiyo amene dzina lake linali Paul anati : “ Munthu aliyense muno akayamba kukuvutitsa , uzikuwa . TSAMBA 20 • NYIMBO : 138 Inu Ndinu Yehova ( nyimbo yatsopano ) , 89 Cofunika kwambili n’cakuti nchitoyo imasangalatsa Yehova amene “ amaona kucokela kosaonekako . ” Yehova analenga Adamu ndi Hava ndi kuwaika pamodzi . Vesi 7 Nkhondo inabuka kumwamba pakati pa Mikayeli ( Yesu Kristu ) ndi cinjoka ( Satana ) . Kodi Cilamulo cinakwanilitsa ciani ? Kupitila mwa mtumiki wake Mose , Yehova anapatsa anthuwo mwayi wosankha kuvomeleza kapena kukana kukhala cuma cake capadela . ( Eks . Anthu ena sangaone mapindu a mphatso imeneyo , koma Akhristu oona amaiona kuti ni ‘ yamtengo wapatali . ’ Ngati tigwilitsila nchito bwino cikumbumtima cathu , cidzatithandiza kucita zabwino ndi kupewa zoipa . Ndimakumbukila ciwawa komanso mikangano imene inalipo m’mabanja ambili m’delalo . Mtsinjewo unalibe madzi patsikuli , koma cinthu cina cinali kunyezimila m’cigwa cimeneco . Mwacitsanzo , ngati muona kuti zimakuvutani kukhululukila ena , pemphani Yehova kuti alimbitse cikhulupililo canu kuti muzikhululukila ena . Koma Mulungu Wamphamvuyonse anaona Eliya mosiyanako . Pamenepa , mwina mungafune kukhala wokhulupilika kwa iye makamaka ngati ndi mnzanu wapamtima kapena wacibale wanu . Mwacitsanzo pali buku ili lakuti “ Khalanibe M’cikondi ca Mulungu . ” M’bukuli muli nkhani ziŵili zokamba za cikwati . 9 : 5 ) Komabe , mwacifundo ca Mulungu , munthuyo anali kuloledwa kuthaŵila ku umodzi mwa mizinda 6 yothaŵilako kuti wobwezela magazi asamuphe . Popeza ndife opanda ungwilo , sitingapewe matenda onse . Munthu angakhale na cimwemwe ngati sali m’cipembedzo conama . Muyenela kuvomeleza kulakwa kwanu m’malo moimba mlandu mnzanuyo . Mwacitsanzo , anayamikila Akhristu a ku Korinto moona mtima pa zimene anali kucita bwino . Ngakhale zinali conco , iye anali kufuna kucita zimene atate ake anam’tuma . Kodi anthu ayenela kucita ciani kuti adzapulumuke cisautso cacikulu ? Panthawiyo , M’bale Rutherford anawalimbikitsa kwambili abale na alongo okhulupilika . 24 : 8 , 9 , 18 , 19 . Zitsanzo zimene tidzakambilana zidzatithandiza tonse kaya ndife acinyamata kapena acikulile kuyamikila zinthu zakuuzimu zimene tinalandila . Nanga kodi munalalikilapo ndi mashelufu a mawilo ? N’zosatheka kukhala na cikhulupililo colimba popanda mzimu wa Mulungu . Mwina angadzifunse kuti , ‘ Kodi ningacite ciani kuti nikapulumuke ? ’ 4 : 8 ) Mulungu amaonetsa cikondi cake mwa zocita . Iye anati : “ Usawelamile milungu yao kapena kuitumikila , ndipo usapange ciliconse cofanana ndi zifanizilo zao , koma uzigwetse ndithu ndi kuphwanya zipilala zao zopatulika . Kodi Mulungu amamva bwanji akaona kupanda cilungamo ? Kodi dzinali limatanthauzanji ? Tingapewe bwanji kusoceletsedwa ndi mabodza a Satana ? Kuyang’ana kwake sikuti kunali kolakwika , koma zinaonetsa kuti anadabwa , ndipo anakondwela ndi kudzipeleka kwa Rabeka . Mu 1991 , Mboni za Yehova ku Russia zinasangalala kwambili zitalandila cilolezo pambuyo pokhala pa ciletso kwa nthawi yaitali . Ponena za mmene zocita za Yesu zinakhudzila anthu padziko lapansi , kodi tingayembekezele kupeza maumboni ena a m’nthawi ya atumwi kuposa a m’Baibulo , amene akuonetsa kuti Yesu anali munthu weniweni ndi kuti anaukitsidwa ? Cikondi ndiye khalidwe lalikulu la Mulungu . Anthu ambili akhala akuikhulupilila kwa nthawi yaitali kupambana mabuku ena . Ndiyeno , panthawi ya mafunso na mayankho , O’Connor uja ndi anzake akufunsa M’bale Russell mafunso amtsutso , koma iye akuikila kumbuyo uthengawo poseŵenzetsa Baibo . Momwemonso cikhulupililo pacokha , ngati cilibe nchito zake , ndi cakufa . ” Ndiponso , cikondi cathu pa Mulungu cimakula tikamasinkhasinkha za nsembe ya dipo imene iye anapeleka kaamba ka macimo athu . MLALIKI 7 : 16 Tiyenela kupewelatu mcitidwe umenewu . Tipewenso kaleya kokonda kuceza mokopana ndi wina amene si m’zathu wa m’cikwati . Kodi makolo ena amakwanitsa bwanji kuphunzitsa ana awo zauzimu mumpingo wa cinenelo cina ? CAKA COBADWA : 1953 Monga okhala m’malo mwa Khristu tikupempha kuti : ‘ Gwilizananinso ndi Mulungu . ’ ” — 2 Akor . “ Citani zonse ku ulemelelo wa Mulungu . ” — 1 AKOR . Anabeleka mwana apo n’kuti mwamuna wake wokondedwa ali na zaka 100 . Conco , ino si nthawi yodziunjikila cuma . Ndipo tisaganize kuti pambuyo pa cisautso cacikulu , tidzakhalabe ndi zinthu zimene tili nazo masiku ano , ngakhale kuti timazikonda bwanji . — Miyambo 11 : 4 ; Mateyu 24 : 21 , 22 ; Luka 12 : 15 . Kodi tikambilana ciani lomba ? Komabe , anthu onsewa anamva uthenga wabwino , anayamba kuphunzila Baibulo , anasintha umoyo wao ndipo ali m’coonadi tsopano . Kazuhiro anati : “ Zimene zinacitikazi zatithandiza kukhulupilila kwambili lonjezo la Mulungu la pa Salimo 37 : 5 , pamene pamati : ‘ Lola kuti Yehova akutsogolele panjila yako , umudalile ndipo iye adzacitapo kanthu . ’ ” Kodi Nsanja ya Mlonda yokhala ndi cingelezi cosavuta yakhala mphatso m’njila yotani ? Iwo ndi odzikuza , odzikonda , ampikisano , ndipo sadela nkhawa zakuti zocita zao zingakhumudwitse ena . Nanga n’cifukwa ciani zinthu zasinthanso ? 6 : 16 - 19 . Amacita zimenezi mwa ( 1 ) kuticenjeza tikayamba kulakalaka zoipa , ( 2 ) kutiongolela tikalakwa , ( 3 ) kutitsogolela ndi mfundo za m’Baibulo , ( 4 ) kutithandiza tikakumana ndi mayeselo , ndi ( 5 ) kutidalitsa akaona zabwino mwa ife . Abale ndi alongo ambili acinyamata asankha kusaloŵa m’banja kapena kusakhala ndi ana kwa kanthawi . Anali kuwatumikila mosewezetsa cuma cake . — Neh . Kodi munacitako ulaliki wa mumseu ? Koma mpukutu wa m’masomphenya a Zekariya unali wolembedwa mbali zonse ziŵili , kuonetsa kuti uthenga wake unali wofunika ngako . 101 - 102 . Kutatsala milungu yocepa kuti ayambe ulendo wake , Eliezere anafunsa Abulahamu za nkhaniyi kuti : “ Bwanji ngati mkaziyo sakabwela nane ? ” Kodi makolo angaphunzitse bwanji ana awo kusankha zovala zolemekezanso Mulungu ? Iye anapempha madziwo mwaulemu ndi modzicepetsa . Mwacitsanzo , taganizilani za munthu amene amacita maseŵela a Olympic . Cotelo , n’zoonekelatu kuti anthu a Mulungu anakhala akapolo a Babulo Wamkulu pambuyo pa caka ca 100 C.E . “ Yehova akhale pakati pa iwe ndi ine , ndi pakati pa ana ako ndi ana anga mpaka kalekale . ” — 1 SAMUELI 20 : 42 . Mavuto amenewa anacititsa kuti iye awadziŵe kwambili malo amenewo . Woyendetsa ngalawa komanso mwiniwake naonso ayenela kuti anali kudziŵa zimenezo , koma ananyalanyaza malangizo a Paulo . Mwadzidzidzi , anam’peza ndi khansa ya m’mapapo imene inafika poipa kwambili , ndipo anauzidwa kuti adzakhala ndi moyo kwa miyezi itatu kapena 6 . Cifukwa cina n’cakuti ‘ sitili mbali ya dzikoli . ’ Cifukwa cakuti anali atavala “ umunthu watsopano , ” Akhristu a m’nthawi ya atumwi anayamba kuona anthu onse kukhala ofanana pamaso pa Mulungu . — Akol . ( Mac 9 : 4 , 5 , 10 - 16 ; 10 : 3 , 4 ; Chiv 10 : 8 , 9 ; 22 : 20 ) Koma kodi amuna amenewa anali kupemphela kwa zolengedwa za kumwamba zimenezi ? ( Mat . 4 : 5 ; Luka 4 : 9 ) , Mar . Kodi mabwenzi abwino angatithandize bwanji kukhala Akristu ofikapo ? MUNGACITENSO IZI Boma limeneli ndilo Ufumu umene Yesu anauza otsatila ake m’pemphelo lacitsanzo kuti aziupemphelela . Iye anawauza kupemphela kuti : “ Atate wathu wakumwamba , dzina lanu liyeletsedwe . Mu Edeni , kodi Yehova anavumbula zinthu ziti zokhudza mdani wathu ? Koma kuti anthu apindule ndi nsembe imeneyi , afunika kumvela Mulungu . Iye anapemphela usiku wonse kwa Atate wake kuti amuthandize kusankha atumwi . Kenako anasankha atumwi ake 12 . Chulani mapindu a kuuzimu ndi akuthupi amene timapeza ngati tiyesetsa kupewa “ kupsa mtima . ” Koma anthu amene amaŵelenga Baibo na maganizo odzicepetsa , ofunitsitsa kuphunzila ngati ‘ tuŵana , ’ amadalitsidwa mwa kumvetsetsa uthenga wa Mulungu . MFUMU SOBHUZA II ya ku Swaziland inalamulila kwa zaka pafupi - fupi 61 . Mwamseli , makolo angakambilane ndi mwanayo mofatsa ndi mwacikondi , na kumufotokozela kuti Yehova afuna kuti iye azilemekeza makolo ake kuti apindule pa umoyo wake . 5 : 4 ) Komabe , amafuna kuti tiziyesetsa kukwanilitsa zosankha zimene tinapanga mogwilizana ndi citsogozo cake . Caciŵili , kumvetsetsa tanthauzo la fanizo limeneli kudzatithandiza kuti tisalefuke cifukwa coona ngati nchito yathu siikuphula kanthu . ‘ Kodi n’zinthu ziti zimene nacita zoonetsa kuti nimam’lemekeza mnzanga wa m’cikwati ? ’ Tidzakhala olimba mtima , tili ndi cidalilo cakuti cipulumutso cathu cili pafupi ( Yoswa 1 : 8 ) Dzifunseni kuti : ‘ Kodi ndili ndi cizoloŵezi cocita phunzilo la Baibulo laumwini ? Mosasamala kanthu za zimenezi , tsiku laulendo litafika , Sara anali wokonzeka kunyamuka . Dongosolo loipali likadzaonongedwa , iye adzaponyedwa m’phompho ndipo adzakhala kumeneko kwa zaka 1,000 . Sadzatelo cifukwa mudzakhala m’mbuyo mwa alendo . M’dzikolo muli zinenelo 120 , ndipo anthu oposa 10 miliyoni amakamba Cinepali , koma ena ambili anangociphunzila . Koma bwanji ngati woyendetsa ndeke wanyalanyaza malangizowo na kutenga njila ina imene iye wafuna ? Kodi nimakhulupilila kuti Mulungu aliko ? Abale a m’Bungwe Lolamulila komanso abale ena a ku likulu lathu , amayendanso pandege kupita ku maiko ena kuti akalimbikitse ndi kuphunzitsa abale nchito zina . ( Yak . 1 : 14 , 15 ) Pamene anali wacicepele , mwina Kaini anali kuona kuti sangapandukile Yehova . 23 : 4 ) Njila imodzi imene Yehova amakhalila nafe ndi kupyolela m’Mau ake . Kodi pali ciliconse cimene mumaona kuti n’cofunika ngako kuposa ubwenzi wanu na Yehova ? Yesu anati : “ Munthu sangakhale ndi moyo ndi cakudya cokha , koma ndi mau onse otuluka pakamwa pa Yehova . ” Imfa sikucitanso ufumu pa iye . ’ 4 : 1 , 2 ) Cikumbumtima caconco cingaticititse kuona ngati “ coipa n’cabwino . ” Kodi kalata ya Yohane ingatithandize bwanji kucita zimenezi ? Tingalimbikitse bwanji mtendele mumpingo ? Popeza kuti Cilamulo cinaletsa Aisiraeli kukwatilana ndi mitundu ya cikunja ndi kulambila konama , colinga cake cinali kuteteza mzele wobadwila wa mbadwa za Abulahamu kuti usaipitsidwe . — Eks . Abale anali kumenyedwa pofuna kuti aulule maina a anthu amene anali kucititsa misonkhano . Baibulo yasintha kwambili malamulo a m’maiko ena , makhalidwe a anthu , ndi zinenelo zambili . Nyumba ya Ufumu ya Wijnegem ikumangidwa m’mbali mwa mseu waukulu m’dela la Antwerp . Kukhulupilila Yehova kudzakuthandizani kuthetsa mantha . M’malo onsewa anali kulimbitsa mitima ya ophunzila ndi kuwalimbikitsa kuti akhalebe m’cikhulupililo . Anali kuwauza kuti : ‘ Tiyenela kukumana ndi masautso ambili kuti tikaloŵe mu ufumu wa Mulungu . ’ ” ( Mac . Alendo ocokela kumaiko ena tingawaonetse kukoma mtima mwa kuŵapatsa moni mwacikondi pa Nyumba ya Ufumu . ( Ŵelengani Genesis 3 : 1 - 5 ; Chiv . Motani ? Mwa zocita zake ndi zimene anali kuphunzitsa , Yesu anathandiza anthu kuzindikila kuti miyezo ya Yehova ni yoyenela , ndi kuti zonse zimene amatipempha kucita zili kaamba ka ubwino wathu . Kwa zaka 15 tsopano , iwo akhala akuthandiza José ndi Rose amene ali ndi zaka za m’ma 80 . 2 : 17 ) Nayenso wamasalimo anaimba kuti : “ Pakuti ocita zoipa adzaphedwa . Koma oyembekezela Yehova ndi amene adzalandile dziko lapansi . Kuti mudziŵe zambili zokhudza mmene mungalimbanilane ndi nkhawa , onani nkhani ya pacikuto ya mutu wakuti : “ Kodi Mumatani Mukakumana ndi Mavuto ? ” mu Galamukani ! Ngati akulu abwela kwa inu ndi kukuthandizani mwacikondi ndiponso mokoma mtima , mwina pankhani ya mmene mumavalila , muzikumbukila kuti malangizo awo ndi umboni wakuti Mulungu amakukondani . Kodi kukhala m’busa kunali ndi zotsatilapo zabwino kwa Mose ? Makonzedwe okhala na mizinda yothaŵilako amaonetsa kuti Yehova ni wacifundo . Komabe , makolo angapindule mwa kuganizila zimene kupanga ophunzila kumatanthauza . Molingana ndi poyamba paja , iye anayang’ananso kwa Yehova kuti am’patse malangizo . Mofananamo , masiku ano abale ndi alongo ambili atumikila Yehova kwa nthawi yaitali , ndipo ndi Akristu ofikapo kuuzimu . 4 , 5 . ( a ) Malinga ndi Salimo 99 , n’ciani cimene atumiki a Yehova amakonda kucita ? Iye anali pa mbali pa Mulungu monga “ mmisili waluso . ” Pokamba za cikhulupililo ca Abulahamu na Sara , onani zimene mtumwi Paulo anauzilidwa kulemba patapita zaka 2,000 . Wacikulile wina amene amakhala mumzinda wa Sofia , m’dziko la Bulgaria , anayamikila kukhala ndi Baibulo la Dziko Latsopano m’Cibugariya . Iye anati : “ Ndakhala ndikuŵelenga Baibulo kwa zaka zambili , koma sindinaŵelengepo Baibulo losavuta kumva ndi lofika pamtima ngati limeneli . ” Pa mbali iliyonse , tidzaona ( 1 ) mmene mbalizo zimatikhudzila masiku ano , ( 2 ) zimene Yehova adzacitapo , ndi ( 3 ) mmene Mulungu adzabweletselapo mbali zabwino . KODI muganiza kuti umoyo ukanakhala bwanji kukanakhala kuti kulibe Baibo ? Maiyo sanakane kuphunzila Baibulo , ndipo anasintha kwambili umoyo wake . Timawayamikila kwambili . ( Ower . Kodi Tingakonzekele bwanji cikumbutso ca imfa ya Yesu caka ciliconse ? Kodi ophunzila a Yesu akhala akukumana na mavuto anji ? “ Citani zimenezi pamene mukumutulila nkhawa zanu zonse , pakuti amakudelani nkhawa . ” — 1 Petulo 5 : 7 . Kudziŵa kwathu zimene Mulungu amafuna ndi miyezo yake , kumatipatsa udindo wocita zinthu zoyenela , na kukweza ucifumu wake . Conco , muzikhala wodekha ndi kupewa kukhumudwa akakupatsani uphungu . 6 : 19 . Mofanana ndi zimenezi , musanaphunzitse m’bale maluso enaake , mungacite bwino kukambilana naye mfundo zolimbikitsa za m’Malemba . N’ciani cingatithandize kudziŵa kuti Mulungu amatiyang’ana cifukwa cotikonda ? * Kucita zimenezi kudzakuthandizani kuyandikila “ Wakumva pemphelo . ” — Salimo 65 : 2 . Iwo anafunikila kucita zimenezo ‘ cifukwa moyo wa nyama iliyonse ndi magazi ake . ’ ( Lev . Mwacitsanzo , ochova njuga mamiliyoni ambili amayembekezela kuti tsiku lina adzawina ndalama zambili , koma sakhala otsimikiza kuti angawinedi . Cifukwa cakuti anali kupita naye kumalo okamunyongela . N’zoona kuti pa nthawi ina , iye anakamba zinthu mosaganiza bwino , koma Yehova anadziŵa kuti anacita izi cifukwa cosautsika mumtima . Mwacitsanzo , ngati pa nyuzi pali nkhani za kuphana , mungakambe kuti : “ Koma anthu ni ankhanza kwambili . Abulahamu anayembekezela mokondwela ngakhale kuti m’nthawi yake sanaone kukwanilitsidwa konse kwa zimene Mulungu anam’lonjeza . M’kupita kwa nthawi , Yehova anapatsa Eliya nchito ina . Iye anakhazikitsa kacisi wamkulu wauzimu , amene ni makonzedwe othandiza anthu kulambila Mulungu mwa nsembe ya Yesu . ( Aheb . Kangapo konse , apolisi anabwela ku nyumbayo . Iwo anali kufuna kudziŵa zimene tinali kucita . Ndi njila yaikulu iti imene Mulungu anaonetsela kuti amatikonda ? Mpaka nthawi imeneyo , kaya ndife amuna kapena akazi , tiyeni tiziyamikila mwai wathu wotumikila Mulungu “ mogwilizana . ” — Zef . Cifukwa ca ziphunzitso zabodza , ena amaganiza kuti Mulungu ndi woipa mtima , ndipo n’zosatheka kum’konda . 13 : 5 ) Tingagwilizanitse mau ouzilidwa amenewa na mau a Yesu olimbikitsa kufuna - funa Ufumu wa Mulungu coyamba na cilungamo cake . ▪ Kodi Mumayamikila Zimene Munalandila ? Fanizolo linaonetsa kuti “ munthu wina wa m’banja lacifumu , ” kutanthauza Yesu , adzafunika kupita kutali kukakhala kumeneko kwa nthawi yaitali asanalandile ufumu . 43 : 10 ) Njila imodzi imene makolo aciisiraeli anacitila umboni , inali mwa kuphunzitsa ana ao zimene Mulungu anacitila makolo akale . Mu 1989 , ine ndi mkazi wanga tinaganiza zobwelela ku Hungary kuti tikauzeko mabwenzi , acibale ndiponso anthu ena zimene tinali kukhulupilila . Pamisonkhano , timalambila Yehova . Mwina tsopano mwamvetsetsa cifukwa cake Yehova anatilamula kupewa “ magazi alionse . ” ( Lev . ( Onani bokosi yakuti “ Zimene Mungacite Kuti Mupite Patsogolo Mwauzimu . ” ) 4 : 6 ) Caciŵili , ganizilani zimene mukakambe mukapita kukakambilana naye . Mwacitsanzo , Marie - Paule wa zaka 74 , wa ku Canada anati : “ Ine ndi mwamuna wanga posacedwapa tinasamuka kucoka m’nyumba yaikulu kupita mu yaing’ono ndipo anzathu ambili anatithandiza . 1 : 7 ) Ndipo ngati mtima wathu ukupitiliza kutiimba mlandu , kodi sizikhala zokhazika mtima pansi kudziŵa kuti , “ Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima yathu ” ? ( 1 Yoh . Cifukwa cakuti analephela kukhulupilila malonjezo a Yehova . N’nali kuonana nawo m’maholide cabe . Ndipo m’cilengedwe conse mudzakhala mtendele . — Aef . Mau amphamvu ndi omveka bwino amenewa a Paulo , aonetsa kuti pamafunika khama kuti munthu akwanitse kuthetsa zilako - lako zoipa . TSAMBA 14 • NYIMBO : 60 , 100 Tinali ofunitsitsa kulalikila uthenga wabwino m’dzikolo . Davide anabweletsa likasa lopatulika la pangano ku Yerusalemu . 5 : 25 ) Kuti otsatila a Yesu atengele citsanzo cake , iwonso afunika kukondana ngati mmene iye anawakondela . ( 16 : 24 ) Kuyambila tsiku limenelo kupita mtsogolo , munthuyo ‘ amakhala wa Yehova . ’ Onani ndime 13 m’nkhani yakuti : “ Kodi ‘ Mudzakhalabe Maso ’ ? ” A Yohane : Koma ndisakubisileni , ine sindikonda zopemphela . Koposa zonse , pemphani Yehova kuti akakuthandizeni kumveketsa bwino mfundo zofunika kwambili za m’Mau ake . — Ŵelengani Ezara 7 : 10 ; Miyambo 3 : 13 , 14 . N’nalandila Coonadi Olo Kuti Nilibe Manja 13 Iwo anali atacoka mumzindawo kwa caka cimodzi , ndipo anayenda ulendo wa makilomita oposa 19,300 , kudutsa m’madela ena akutali kwambili a miyala m’dzikolo . Kodi io adzadalitsika motani ? Ngakhale kuti mkazi wa Potifala anam’kakamiza kwa nthawi yaitali , Yosefe anasankha kumvela Mau a Yehova osati a mkaziyo . Taona kuti mau apa Salimo 34 : 8 ndi oona . ( 1 Akor . 10 : 6 - 11 ) Pa mayeselo amenewo , palibe ciyeso cimodzi cimene cinali cacilendo kwa anthu kapena cimene Aisiraeli okhulupilika sakanatha kupilila . N’cifukwa n’ciani tingakambe kuti munthu aliyense amene akupita kukabatizika amakhala atadzipeleka kale kwa Yehova na mtima wonse ? 4 : 10 , 11 ) Cikondi cimene Akristuwo anali naco kwa Paulo cinali kuwasonkhezela kumutonthoza ndi kumulimbikitsa pakafunika kutelo . Mwacitsanzo , nthawi ina Mfumu Sauli anacita zimene anaganiza kuti ni cifundo , koma kunali kusamvela Mulungu . Iye anapempha Sauli kuti akadye naye cakudya m’cipinda codyela . ( 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 ) Tiyeni tione mavuto atatu amene amabwela cifukwa cokoka fodya ndi zimene Baibulo limanena . KULEKA KUKOKA KUMAVUTA Dzinali linali kulembedwa ndi zilembo za Ciheberi zinai izi : יהוה zimene zimalembedwa kuti YHWH Anacitanso cimodzi - modzi poyesa Yesu . ( Mat . Cinsinsi Namba 3 Kulemekezana Pamene asilikali anali kuomba mfuti , zipolopolo zinali kudutsa pafupi na ine . Koma zombozo zinasweka cakuti sanathenso kuzigwilitsila nchito . — 2 Mbiri 20 : 35 - 37 . Mwamsanga , Baraki anapita kukamenyana ndi adani ake monga mmene Yehova anam’lamulila . Sisera ataphedwa , Mfumu Yabini sinavutitsenso Aisiraeli . Ndipo anthu mamiliyoni amene amaphunzila nafe Baibulo ali ndi zipembedzo zao . Nthawi zina , atumwi anali kukangana pankhani ya amene anali wamkulu pakati pao . Mwacitsanzo , mu Galamukani ! Iye anati : “ Tsopano ndacita upainiya kwa zaka zitatu . Atate a anawo anakamba kuti : “ Ana athu asanayambe kuyenda na kukamba , tinali kuwauza za cimwemwe cimene munthu amakhala naco ngati acita upainiya ndi kutumikila mumpingo . Pamene Paulo anawacezelanso , anaona kuti Timoteyo angawathandize kwambili pamaulendo ake aumishonale . Cinanso , anzathu a m’dziko limene tinacokela anali kutitumila mameseji pa kompyuta na makalata otilimbikitsa kuti tipitilize utumiki wathu . ” — Afil . Yesu pogwilitsila nchito mphamvu za Yehova anaukitsa bwenzi lake , ndipo zimenezi zinaonetsa kuti iye ndi wacifundo kwambili . — Yoh . 11 : 43 , 44 . Ngakhale n’telo , nkhondo ikalipo ndipo nthawi zina tingatope polimbana ndi adani athu amenewa , kapena cifukwa coona kuti mapeto a dziko loipali akucedwa . Anthu m’nthawi ya Yesu anali ogaŵikana cifukwa cosiyana pa zandale , cikhalidwe , kapena mitundu . Aksamai anapita kwa Elizabeth kukasoketsa zovala . Iye anafunsa Elizabeth mafunso ambili okhudza colinga ca moyo komanso mkhalidwe wa akufa . Yakobo kuyambila paciyambi anakonda kwambili Rakele amene anali wokongola . Mwacitsanzo , Corrado wa ku Italy , wa zaka 77 anati : “ Mukamayendetsa galimoto pokwela makata mumasintha magiya osati kuzimitsa galimotoyo . Titayenda makilomita ambilimbili , tinafika pakati penipeni pa nyanja . Tili aŵiliŵili m’boti laling’ono pakati pa nyanjapo , ndi pamene ndinazindikila kuti ndine wamng’ono kwambili kuyelekezela ndi Mlengi wathu wamkulu . 32 : 3 - 5 ) Conco , ngati munacita chimo lalikulu , dziŵani kuti Yehova ni wokonzeka kukuthandizani kukonzanso ubwenzi wanu na iye . Koma ndikuona kuti kudzipeleka kwa Yehova ndikali wamng’ono kunandithandiza kuti ndisayambe kufunafuna zinthu za m’dzikoli . ” Cifukwa cakuti io afuna kuti wacibaleyo adziŵapatsa ndalama . ( Miy . 19 : 6 , 7 ) Anna anati : “ Ngakhale n’conco , tikapewa kuika zinthu zakuthupi patsogolo acibale ena m’kupita kwa nthawi angazindikile mmene kuika zinthu za kuuzimu patsogolo kulili kofunika . Ngakhale n’conco , ciyembekezo cokhala ndi moyo kwamuyaya sicidalila sayansi . Ngakhale masiku ano , anthu akugwilitsilabe nchito luso limeneli m’malo ena . Ndiyeno ananditumiza ku ndende ya Kachere kumene ndinakhalako miyezi isanu . Ndiyeno , anthuwo anamukokela kunja kwa mzindawo poganiza kuti wafa . — Machitidwe 14 : 19 . MUZIPILILA . ( Ŵelengani Machitidwe 1 : 6 - 8 . ) ( 1 Sam . 1 : 12 , 17 , 18 ) Hana anali kukhulupilila kuti Yehova adzathetsa vuto lake la kusabala kapena adzamuthandiza mwa njila ina . “ Dzanja la Yehova lidzadziŵika kwa atumiki ake . ” — YESAYA 66 : 14 . Pamenepo iyo idzapita ndi ukali waukulu kuti ikafafanize ndi kuwononga ambili . Ndipo idzamanga mahema okhala ngati nyumba yacifumu pakati pa nyanja yaikulu ndi phili lopatulika la Dziko Lokongola . 12 ) Zioneka kuti Demetiriyo anali kufunikila thandizo la Gayo , ndipo kalata yacitatu imene Yohane analemba iyenela kuti inalinso njila yodziŵikitsila Demetiriyo kwa Gayo kuti ndi Mkhristu wacitsanzo cabwino . Anali kuzondanso uthenga wake ndi Mulungu amene anam’tuma . ( Aroma 10 : 4 ) Kenako , Yesu ananenanso kuti : “ Nthawi . . . ndi yomwe ino . ” Kodi ndi cosankha cofunika kwambili citi cimene muyenela kupanga ? Ndi cosankha cotumikila Yehova . 6 : 14 . Ndani anakhala anthu apadela a Yehova ? Nanga n’ciani cinawasiyanitsa ndi anthu ena ? Anali ataona mbuye wawo ndi mnzawo , Yesu , atakwela kumwamba ndi kubisika m’mitambo . Kuti ziphuphu zithe , anthu afunika kuphunzitsidwa kuti adziŵe mmene angathetsele mtima wa dyela ndi wodzikonda . Kodi mungalimbikitse bwanji mwana wanu wacinyamata kuti aongolele ? Tidzaphunzila mmene Akristu masiku ano , angaonetsele kuti ‘ amadziŵika ndi Yehova , ’ ndi kuti ‘ aleka kucita zosalungama . ’ Naboti anali kudziŵa kuti Ahabu ndi munthu woopsa , koma iye analankhula naye cifukwa anali ndi cikhulupililo colimba ndiponso wolimba mtima . Ŵelengani Luka 16 : 1 - 9 . Iyai . Popeza Yesu analibe chimo , ndipo anali “ wopanda cilema , ” iye sanali kufunikila kuyeletsedwa . ( Aheb . Tingaphunzile mfundo zofunika pa citsanzo ca Robert . ( Mateyu 7 : 13 , 14 ) Mosakaikila , kuti tiyende pa njila imeneyi tingapindule kwambili kukhala pafupi na wotitsogolela wodziŵa bwino njila imeneyo kuti tikafike kumene tiyenda , kumene ni ku moyo wosatha . Koma panthawiyo , Paulo analimbikitsa abale kuti ayenela kukondana kwambili . Aliyense wa ife ayenela kudziŵa kuti sangakwanitse kucita zonse potumikila Yehova . Ribeiro anacoka panyumba ali na zaka pakati pa 13 ndi 19 , ndipo m’kupita kwa nthawi anakaloŵa nchito pa fakitale ina yopanga mapepa kucokela ku mabuku amene amataidwa . Komanso Malemba amati “ mu Isiraeli simunakhalebe mneneli aliyense wofanana ndi Mose , amene Yehova anali kumudziwa pamasom’pamaso . ” Ku Harana , banja limeneli linakhalako kwa kanthawi . Pulofesa wina wa maphunzilo a zacipembedzo anati : “ Sitidziŵa ngati tamasulila Baibulo molondola mogwilizana ndi mipukutu yoyambilila . Pamene Yehova anauza Abulahamu ndi banja lake kuti acoke ndi kupita ku Kanani , iye anamvela ndi mtima wonse . Kodi panyumba panga na katundu wanga zimakhala zaukhondo nthawi zonse ? 4 : 4 ) Conco , akulu akakupatsani uphungu woyenelela wocokela m’Baibulo , yesetsani kuulandila ndi mtima wonse , ndipo gwililamponi nchito . Conco , munthu amene amatumikila Yehova na mtima wake wonse sacita zinthu mwaciphamaso . Kodi nchito yolalikila inali yofunika motani kwa Yesu ? Yesu anali kuyenda m’madela osiyanasiyana kukalalikila . Yesu anali kuyesa kupeza njila zotonthozela ena ndi kuwathandiza . Kodi anamva manyazi poona kuculuka kwa zopeleka za ena amene anali patsogolo pake , ndi kuganizila kuti mwina copeleka cake cinali ca cabe - cabe ? Ndipo cifukwa conyada , Sauli anapanga cipilala ca cikumbutso cake . Ndipo akatswili ena a Baibo amakamba kuti lamuloli linali lofunika ndi loyenelela . N’zoona kuti ambili a ife sindife akapolo ndipo sitigwila nchito yaukapolo . Za cikondi cimeneci , mtumwi Paulo anati : “ Aliyense wa inu akonde mkazi wake ngati mmene amadzikondela yekha , komanso mkazi azilemekeza kwambili mwamuna wake . ” — Aef . Nthawi zina , ofalitsa nkhani amakometsa mbali imodzi pokamba nkhani zao . Ni wapadela . Nanga Baibo itanthauza ciani pamene ikamba kuti Inoki “ anasamutsidwa kuti asafe mozunzika ” ? Koma m’kupita kwa nthawi , iye analephela kukhala wokhulupilika kwa Yehova monga munthu wauzimu . M’malo mocosapo vuto lathu , nthawi zambili Mulungu amatipatsa mphamvu kuti tipilile vutolo . Anacita izi kuti atsimikizile kuti Timoteyo waphunzitsidwa bwino . M’CILAMULO CA MOSE , kulumbila nthawi zina kunali koyenelela . Iye akuona mavuto amene m’bale wacikulileyo akukumana nao ndipo akumumvetsela mokoma mtima . Conco , tiyenela kuona nchito yathu monga njila yabwino yotithandiza kukwanilitsa zolinga zathu ndi udindo wathu . ( 2 Mbiri 6 : 32 , 33 ) Mofananamo , m’nthawi ya Yesu anthu osakhala Aisiraeli koma amene anali kufuna kulambila Yehova , anafunika kugwilizana ndi anthu a Mulungu . — Yoh . 12 : 20 ; Mac . Amatiuza mmene tingasankhile munthu wokwatilana naye , ndi mmene tingakhalile mkazi kapena mwamuna wabwino . Mlongo wina wokwatiwa amene akutumikila ku likulu ku New York , anakamba izi ponena za gulu la Yehova : “ Ndilo gulu lokha limene limalengeza dzina la Yehova mokhulupilika . Ngati tifunitsitsa zinthu zimenezi , tingayambe kuzikonda kwambili kuposa mmene timakondela Mulungu . Unaseka iwe . ” — Genesis 18 : 9 - 15 . Koma Mose sanagonje , ndipo molimba mtima anasankha kucilikiza kulambila koona . Ndiye ndingakwanitse bwanji kumvetsetsa Baibulo Lopatulika ? ” ​ — AMIT , INDIA . Ni mfundo yakuti : Yehova adzacititsa kuti onse amene amamulambila akhale ‘ amodzi . ’ ( Ezek . 16 , 17 . ( a ) Kodi Yehova afuna kuti anthu ake azicita ciani ? Kudzifufuza n’kofunika . Ndipo zinthu zikuluzikulu zimene zakhala zikucitika padziko lapansi kuyambila cakaco , zikutitsimikizila kuti Ufumu wa Mulungu unayambadi kulamulila mu 1914 . Ndipo mu utumiki wake wa padziko lapansi , Yesu anali kufotokoza maganizo ake kwa Atate ake akumwamba kupyolela m’pemphelo . Ali na zaka 15 , anagwa mu mtengo ndipo ziwalo zake zinazizila kuyambila m’khosi mpaka ku mendo . Patapita nthawi , mavuto ake anatha ndipo anakhala wokondwela . Ziphunzitso monga cisanduliko zimatenga cilengedwe kukhala mulungu , ndi kucipatsa mphamvu zimene kweni - kweni n’za Yehova yekha . M’zikhalidwe zina , makolo ndi amene amasankhila mwana wao munthu wokwatilana naye , ndipo okwatilanawo samadziŵana mpaka pa tsiku la cikwati . Ndife otsimikiza kuti pamene muphunzila ndi kupindula na mphatso yopambana zonse imeneyi mudzalimbikitsidwa kufuula kuti : “ Ndiyamika Mulungu , mwa Yesu Kristu Ambuye wathu ! ” — Aroma 7 : 25 . ( Buku lopatulika ) Ndipo ndinadziona kukhala wamlandu ndi wosafunika . ” Ndinakhala wolemekezeka kwambili m’gulu la zigaŵengalo cifukwa ca ukali umene ndinali nao . 13 : 34 , 35 ) Ana amakumbukila bwino zinthu zocitika . YESETSANI KUKHALA NDI NDANDANDA YOKHAZIKIKA 1 : 19 - 21 ) Ngati tingamwalile tili okhulupilika Aramagedo isanacitike , tidzaukitsidwa m’dziko latsopano lolungama . Nikhoza kucita zambili mu utumiki wa Yehova kuposa mmene nicitila tsopano . ’ “ Mulungu alibe tsankho . Iye amalandila munthu wocokela mu mtundu uliwonse , amene amamuopa ndi kucita cilungamo . ” 61 : 8 ) Mwacitsanzo , ngati mwamuna kapena mkazi ku nchito kapena kusukulu wayamba kutifuna , kodi timakana pofuna kuonetsa kuti ‘ timasangalala na njila [ za Yehova ] ’ ? Munthuyo anapindula kwambili ndi thandizo lanu , nanga kodi nanunso munapindula ? Kodi inuyo mwatsimikiza mtima kucita ciani panchito yolalikila ? Ubatizo sucotsa macimo , koma umaonetsa kuti munthu wadzipeleka kwa Yehova Mulungu ndi mtima wonse . Kuyambila paciyambi , anthu akhala akupanga zosankha pa nkhani zazikulu . Anthu amene sali pabanja angacite zambili mu utumiki , cifukwa sakhala ndi nkhawa zimene anthu ali m’cikwati amakhala nazo . — 1 Akorinto 7 : 32 - 35 . Lemba la Aefeso 2 : 7 likamba kuti Mulungu adzaonetsa kukoma mtima kwakukulu “ mu nthawi zimene zikubwela . ” Mau akuti “ m’kamwa mwa mkango ” amene Paulo anagwilitsila nchito angatanthauze mkango weniweni kapena wophiphilitsila . Komabe , mau ake anali acikale ndi ovuta kumva . Gulu la Yehova lapeleka zida zambili zimene makolo angaseŵenzetse pophunzitsa ana awo . kusintha - sintha kwa zinenelo ? Ndipo taphunzila kusonyeza kudzicepetsa ngakhale kuti nthawi zina zimakhala zovuta . ” Mmene Yapulumukila , Na . ‘ Nzelu Zopindulitsa , ’ Oct . Mtumwi Paulo anacenjeza kuti “ kudziŵa zinthu kumacititsa munthu kudzitukumula . ” Yesu amagwilitsila nchito mzimu woyela potsogolela mipingo . Ndiyeno , magetsi atabwela , iye anayamba kuŵelenga nkhani yokamba za Mwambo wa Omaliza Sukulu ya Giliyadi mu Nsanja ya Olonda . Inde , makolo amene akhala m’dziko lina , afunika kupeza nthawi yokwanila yothandiza anawo kukhala pa ubale wolimba na Yehova . Afunikanso kupeza njila zosiyana - siyana zowathandizila . Makolowo angacite mantha poganiza kuti akadzakalamba , mwana wawo sadzakwanitsa kuwasamalila . Kingsley anayankha kuti : “ Iyai , ndakhala ndikuyeseza maulendo 30 tsiku lililonse . ” Yehova analamula Adamu na Hava kuti abeleke ana na kudzaza dziko lapansi , komanso kuti azilisamalila . Ndiye cifukwa cake tiyenela kucita zimene tingathe kuti tizipezeka pamisonkhano ndi kulandila thandizo la Mulungu kudzela mwa mzimu wake . Mungatengele bwanji citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wozindikila ? Ganizilani izi : Ponena za nthawi imene Gogi adzagonjetsedwa , Yehova anakamba za iye kuti : “ Ndidzakupelekani kwa mbalame zodya nyama , mbalame zamitundumitundu ndi zilombo zakuchile kuti mukhale cakudya cao . ” ( Ezek . Kodi uthenga wa Zekariya unawakhudza bwanji Ayuda a m’nthawi yake ? Conco , masiku ano mumpingo wacikristu simuyenela kukhala magaŵano a mtundu uliwonse . — 1 Akor . 1 : 10 - 13 ; ŵelengani Aroma 16 : 17 , 18 . Ubale wanu ndi Yehova udzalimba kwambili pamene mupitiliza kupilila mosasamala kanthu za ziyeso zimene mungakumane nazo tsiku lililonse . Pali mau ena amene tinali kukonda kukamba akuti “ Khala mbeta mpaka utakwanitsa zaka 23 . ” Lolani kuti Yehova akuyengeni . Pa zonse zimene zinamucitikila , iye anakamba kuti , “ N’naona dzanja lacikondi la Yehova . ” Koma pang’onopang’ono coonadi cinali kuzika mizu m’mitima yathu . Esitere caputa 2 - 5 , 7 - 9 ( b ) Nanga ‘ tingamuyang’anitsitse ’ bwanji Yesu ? Kodi a nkhosa zina ayenela kudziŵa maina a odzozedwa onse amene akali padziko lapansi masiku ano ? Nanga zimenezi zimasonyeza ciani ? Mphamvu za Yehova zinathandiza Yesu Kristu kucita zozizwitsa zambili . Zimenezi zapangitsa kuti anchito ambili azikhala na nkhawa ndiponso azikhala olema . Anali kuganiza na kucita zinthu motengela Yehova . Izi zingaoneke ngati zazing’ono , koma zingalimbikitse munthu , ngakhale amene ni wopanikizika maganizo kapena wokhumudwa . Koma usiku anali kuzitsekela m’khola pofuna kuziteteza ku zilombo zolusa , ku akawalala , ndiponso kuti zikhale mothuma . Cinanso , tinaphunzila kuti Ufumu wake udzathetsa mavuto onse , ndi kuti tili na ciyembekezo codzakhala na moyo wosatha , mwamtendele ndi mosangalala mu Ufumuwo . — Yoh . Njila imene Lefèvre anali kutsatila pomasulila Malemba inathandiza ngako akatswili ena a Baibo ndi anthu ena otsutsa ziphunzitso za chalichi ca Cikatolika . — Onani bokosi yakuti “ Mmene Zolemba za Lefèvre Zinakhudzila Martin Luther . ” Motelo ngati mufuna kuloŵa m’banja tengelani citsanzo ca m’busa ndi Msulami . Iye adzakhala weniweni kwa inu . 10 : 1 . Kumeneko mudzamanga guwa la nsembe . ” Koma n’zacisoni kuti nthawi zina timalephela kum’kondweletsa cifukwa ndife opanda ungwilo . Conco , zinali zosavuta kuti anthu a mumzindawo azithandizana ndi kutetezana pakakhala mavuto . Baibulo imatiuza kuti , “ musamade nkhawa ndi kanthu kalikonse koma pa ciliconse , mwa pemphelo ndi pembedzelo , pamodzi ndi ciyamiko , zopempha zanu zidziŵike kwa Mulungu . Colinga cimodzi ca sukulu imeneyi ndi kuthandiza ana a sukulu kukonda nchito yolalikila uthenga wabwino . Ponena za paladaiso wauzimu , ndi mwai wotani umene tili nao ? Mwacitsanzo , Petulo anakamba kuti sangamusiye Yesu ngakhale anzake ena onse atathawa . Kumeneku ndiye kunali kwawo kwa mneneli Samueli . Delali linali pamtunda wa makilomita 35 kum’poto cakum’madzulo kwa Yerusalemu . — 1 Sam . Komabe , midzi imeneyo inali yosiyana ndi kumene Sara anakulila . Ndipo anaonetsa kuti munthu wangwilo angathe kukhalabe wokhulupilika kwa Mulungu ngakhale panthawi ya mavuto . Koma silitilangiza kuti tiyenela kuona munthu wina aliyense monga mtsogoleli wathu . ( 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 ) Koposa zonse Baibo ili na malangizo amene amathandiza nthawi zonse , malangizo amene sasila nchito . Abale ena anacokela ku dziko la United States , limene lili kutali ndi dziko la Japan , kuti akathandize abale athu . Conco ndinayamba kukondwela kwambili kuuza ena za Atate wathu wakumwamba , amene ndi wacikondi ndipo amakhululukila ndi mtima wonse . ( Mat . 4 : 1 ; 6 : 13 ) N’cifukwa ciani Yehova analola zimenezi kucitika ? Makhalidwe amene anafotokozedwa pa lembali ali ponse - ponse m’dzikoli . Kucita zimenezi kunali monga kuti wafika kwa Mulungu . ( Lev . Mkazi wina wosauka anavutika ndi matenda oopsa kwa zaka 12 . Komanso anthu ambili sanali kumvetsetsa kafotokozedwe kakale kokhudza zocitika za m’Baibulo ndi zinthu zimene zinali kuimila mtsogolo . Mafumu okhulupilika amenewo anali osiyana kwambili ndi atsogoleli a mitundu ina amene anali kutsogoleledwa ndi nzelu za anthu zosathandiza konse . Kodi Baibulo limayankha bwanji ? Tikakhala muulaliki , kodi tingathandize bwanji anthu ena kukhala mabwenzi a Yehova ? N’cifukwa ciani Baruki anasoŵa cimwemwe ? Nanga Yehova anamupatsa uphungu wotani ? Ngakhale n’conco , n’zotheka ndithu kuonetsa khalidweli . Abale na alongo anapitiliza kumukomela mtima . Zimenezi zinamuthandiza kupita patsogolo mwauzimu . Ena anali kugona m’Nyumba za Ufumu . Zizindikilo zoonetsa kuti munthu wakhala pafupi kumwalila zandandalikidwa pa bokosi lakuti “ Wodwala Akakhala Pafupi Kumwalila . ” Mulimonse mmene zinalili , Yosefe ayenela kuti anakhumudwa kwambili na kupanda cilungamo kwakukulu kumeneku . Koma palibe zimene akanacita . Russell . Uwu unali ulendo wake wacisanu wopita ku Ireland . Hava atangolengedwa , Adamu anamuuza lamulo la Mulungu . Kuwonjezela apo , wopeleka mphatso angacite bwino kudzifufuza kuti adziŵe colinga cake . “ Ana athu amafunika kuona kuti timavomeleza tikalakwitsa komanso timapepesa . Ndipo cikondi “ cimakhulupilila zinthu zonse , ” za m’Baibulo ndi kuticititsa kuti tiziyamikila cakudya ca kuuzimu cimene timalandila . Pamene Asa anaopsezedwa ndi ufumu wa Isiraeli wakumpoto , iye anapempha thandizo kwa a Siriya . Koma akapanda kumumvela , anali kukumana ndi mavuto aakulu . — Ŵelengani Deuteronomo 28 : 1 , 2 , 15 . Kukalamila maudindo mumpingo ndi dalitso locokela kwa Yehova . Ndingacite ciani kuti ndizidalila kwambili Yehova ? Komabe , cikodi ca a·gaʹpe “ cimakwilila zinthu zonse , cimakhulupilila zinthu zonse , cimayembekezela zinthu zonse , cimapilila zinthu zonse . ” Komanso , olandila alendowo anayamikila kwambili khalidwe labwino la abale ocokela m’maiko ena . M’loto loyamba , mfumuyo inaona ng’ombe 7 zikutuluka mumtsinje wa Nailo , ndipo ng’ombezo zinali zokongola m’maonekedwe ndi zonenepa . Magulu a apainiya analimbikitsidwa kukhala pamodzi na kulalikila mogwilizana , kuti asamawononge ndalama zambili . Felike anali kulamulila Yudeya , ndipo panthawiyi anali atamvapo kale zimene Akhiristu amakhulupilila . Afunseni zokhudza banja lawo . * Conco , n’nali na zitsanzo zabwino zambili zimene ningatengele . Kodi imwe mufuna kupitiliza kupita patsogolo ? Buku lina lokamba za umoyo wa anthu a m’nthawi ya Yesu limati , “ magulu a cipembedzo aciyuda anali kucita zinthu mofanana ndi zipani zandale ” ( Daily Life in Palestine at the Time of Christ ) . Kubatizika kumatsegula mwayi wolandila madalitso ambili , koma kumabweletsanso udindo . 4 : 3 - 16 . Tsopano , tiyeni tikambilane njila zimene zingatithandize kutengela Yesu . Kodi Yehova ni Woumba wamkulu m’njila ya bwanji ? Kodi Yehova amatithandiza bwanji kuti tikwanilitse utumiki wathu ? Ngati makolo ndi ana sakhala pamodzi monga banja , cikondi cao cingacepe ndipo khalidwe lao lingaonongeke . ( Yes . 55 : 11 ) Ifenso tiyenela kukhulupilila kuti Yehova adzakwanilitsa lonjezo lake lakuti : “ Sindidzakusiyani kapena kukutayani ngakhale pang’ono . ” ( Aheb . Ni kudya vakudya vopatsa thanzi , kucita maseŵela olimbitsa thupi , na kukhala na makhalidwe abwino . 1 , 2 . ( a ) Atatsala pang’ono kuphedwa , kodi Yesu anawauza ciani ophunzila ake ? Mwacionekele , anafuna kuti anawo asadzaukile m’bale wawo Abiya , amene anali kudzakhala mfumu pambuyo pa imfa yake . Zoona , Yehova adzaonetsetsa kuti tili ndi zinthu zofunikila mu umoyo . Tinali kuopa kugula zinthu pa nkhongole cifukwa coganiza kuti makampani satilola kugula pa nkhongole . M’kupita kwa nthawi , Matthew anayamikilidwa kukhala mkulu komanso mpainiya wapadela ndipo tsopano akutumikila pa ofesi ya nthambi pafupi ndi mzinda wa St . Kodi acicepele angazindikile bwanji phindu la mfundo za m’Baibulo ? Ngati ndinu m’bale , kodi mungaphunzitse abale acinyamata mmene angapelekele nkhani zolimbikitsa ndi kukhala alaliki ogwila mtima a uthenga wabwino ? Atumiki a Mulungu padziko lonse amafuna kuvala na kudzikonza moyenelela . Amavala zovala zooneka bwino , zoyela , ndi zololeka kudela la kwawo , komanso zogwilizana ndi mfundo za m’Malemba . Satana amayesanso kutinyenga mwa njila ina . NYIMBO : 53 , 107 Kodi ndi vuto liti limene ana osamalila makolo angakumane nalo ? Kodi mukanakhala imwe , sembe munakwela basi iliyonse cifukwa coona kuti anthu ali m’basimo akuoneka okondwela ? M’malomwake , anali kuwacondelela . Tidziŵa bwanji kuti tonse tingathe kubala zipatso pa nchito yathu yolalikila ? ( Aroma 5 : 12 ) Tingam’fotokozelenso kuti Mulungu sanamuuze kuti adzalandila cilango m’moto wa helo . N’cifukwa ciani Yehova watilola kukhala “ anchito anzake ” ? Iye anati : “ Popanda cikhulupililo n’zosatheka kukondweletsa Mulungu . ” Khalani woceleza . Iye analemba kuti : “ Zimene zinacitikazo zinanithandiza kuzindikila kuti Yehova amatikonda . Salimo 119 : 21 imakamba za Yehova kuti : ‘ Mumadzudzula odzikuza . ’ Ataona kuti Mariya wamulekelela , Marita anakhumudwa cakuti anadandaulila Yesu . Pitiliza kuphunzila Baibulo . ’ Komabe , pakhalako masinthidwe ena okhudza nkhani imeneyi . Zinalidi zosangalatsa kwambili kugaŵila anthu zofalitsa m’cinenelo cao ! Umoyo wathu wa pa famu titangokwatilana N’cifukwa ciani Malemba amakamba kuti mkwatibwi ali pa “ ulemelelo waukulu ” ? Anamupempha kuti amutsegulile njila kuti apitilize kutumikila monga mpainiya . Kwa zaka zambili , Ophunzila Baibulo a ku Pittsburgh anali kucita misonkhano yacigawo ya okhulupilila dipo amene anali kubwela ku Cikumbutso . Koma tsiku lina pamene n’nali mu ulaliki na mkulu wina , anaona kuti sin’nali wokondwela . Mwacitsanzo , ganizilani zimene zili m’buku la Yesaya . Tikamva njala , mwina timatenga mkate ndi kudya . Okalamba ayenela kupatsiwa gawo lowayenelela . Yehova amacita zinthu zabwino kuposa kupeleka zikwangwani za malangizo ocenjeza . Mtundu wa anthu sudzanyamula lupanga kuti umenyane ndi mtundu unzake , ndipo anthuwo sadzaphunzilanso nkhondo . . . . ndipo sipadzakhala wowaopsa . ” Ife tasiya zinthu zonse ndi kukutsatilani , kodi tidzapeza ciani ? ” Ndipo akatswili amakamba kuti pofika m’nthawi ya atumwi , Ayuda oposa 60 pelesenti sanali kukhala m’dziko la Isiraeli . Ha ! ikomelenji mphoto yake — moyo na mtendele ! ( Mateyu 22 : 37 ) Ndithudi , Mulungu afuna kuti tizigwilitsila nchito bwino moyo wathu ndi matupi athu ndi kuzisamalila . Conco musamade nkhawa n’kumanena kuti , . . . Pamene ndinatsimikiza kuti dzina la Mulungu ndi Yehova , ndinayamba kuona kuti payenela kuti palinso zinthu zina zimene sindinali kudziŵa . ” Ndithudi , zozizwitsa zimene Yesu anacita zimasonyeza kuti iye amakonda anthu . ( Ŵelengani Yesaya 40 : 12 - 15 . ) 5 : 16 ) Zaka 100 zapitazo , abale athu anali okangalika ndipo anacita zambili potumikila Yehova . Koma zimativuta kupeza nthawi yoŵelenga zofalitsa zonse zimene talandila . 11 : 1 - 21 ) Chimo la Davide silikanabisikabe . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Musamaganizile zofuna zanu zokha , koma muziganizilanso zofuna za ena . ” — Afilipi 2 : 3 , 4 . Ndipo zimenezi ndi zogwilizana ndi mfundo ya m’Baibulo yakuti : Ndinu amtengo wapatali pamaso pa Yehova . Ndipo lemba la Afilipi 2 : 12 , limati : “ Pitilizani kukonza cipulumutso canu , mwamantha ndi kunjenjemela . ” Anthuwo anagwilitsilanso nchito nthawi yao ndi mphamvu zao pa nchitoyo . Kudzatithandizanso kum’tumikila ndi mtima wonse ndi kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu mwacangu . ( Mat . Kodi kukambilana zimenezi kudzatithandiza bwanji ? Kodi mukumbukila zimene zinacitikila Kaini pamene anakwiila kwambili m’bale wake cifukwa ca nsanje ? 22 Mungakhalebe Wodzicepetsa pa Mayeselo ( b ) N’cifukwa ciani tifunika kusamalila Nyumba ya Ufumu nthawi zonse ? Kodi mkate ndi vinyo zimaimila ciani ? Kodi kuuzako munthu amene mumam’dalila nkhawa zanu kungakuthandizeni bwanji ? Motelo , wina akalakwa , tiyeni tizionapo mwayi wotengapo phunzilo pa colakwaco , wokhululukilana , ndi wosonyezana cikondi monga ‘ cogwilizanitsa camphamvu . ’ ( Akol . Koma pali njila zambili zoyambila makambilano . Oyang’anila dela , abale a m’ma Komiti a Nthambi , amishonale , ndi abale ena amayenda pandege kuti akakambe nkhani ku misonkhano yacigawo ndi kulimbikitsa mipingo . Iye ananilangiza kuti niphunzileko luso linalake limene lidzanithandiza pocita upainiya . N’nali kusungulumwa kwambili . ” Cifukwa Cake Tifunika Kupulumutsidwa 8 ( Mat . 24 : 42 ) Musakhulupilile bodza la Satana lakuti mapeto ali kutali kapena kuti sadzabwela . Alongo , ana awo , ndi ophunzila Baibo anga , ananithandiza moleza mtima kuti niphunzile citundu cawo . Ndipo kuyambila mu July 1994 , ndakhala ndi mwai wotumikila m’Bungwe Lolamulila . 28 : 2 . Ofalitsa akanaleka kulalikila , sembe ku Khoti Lalikulu kulibe milandu . Koma popeza inu ofalitsa , abale padziko lonse simunaleke kulalikila , n’cifukwa cake tagonjetsa anthu amene akutizunza . ku nchito ? Kodi cikhulupililo ca Paulo mwa Yehova cinalimba bwanji ? Pamene akaidiwo anamasulidwa , ambili anabwela m’dziko la Kyrgyzstan , ndipo ena mwa iwo anabwela na coonadi . 9 : 11 ) Kodi anagona m’cipinda cimodzi kapena zosiyana ? Kodi Yesu wagwilitsila nchito motani Ufumu wa Mesiya poyenga , kuphunzitsa , ndi kulinganiza atumiki okhulupilika a Mulungu padziko lapansi ? “ Ufumu Wanu Ubwele ” — Kodi Udzabwela Liti ? [ Mau apansi ] Kapena kuti “ amatilimbikitsa . ” Atumiki a Yehova okhulupilika akale anacitapo macimo aakulu , koma Mulungu sanawasiye . 4 : 29 , 30 ; 11 : 4 - 6 ) Conco , kuwonjezela pa kukhala na cidziŵitso ca m’Baibo , tifunikanso kupitiliza kupita patsogolo mwauzimu . ( Akol . ▪ Muziyamikila Mwai Wanu Wogwila Nchito ndi Yehova N’zomveka kufunsa mafunso monga awa : ( Mac . 2 : 22 ) Zozizwitsa zimene Yesu anacita zimapeleka cithunzi ca madalitso osaneneka amene tidzalandila mu ulamulilo wake . Kukamba zoona , Sara sanali kuyembekezela ngakhale pang’ono kuti angabeleke mwana , Isaki . — Gen . Nthawiyo ndinali ndisanamvepo coonadi . Mwacitsanzo , zomela zimalandila mphamvu ya dzuŵa , ndipo zimagwilitsila nchito mphamvuyo kusintha mpweya wa carbon dioxide , madzi , ndi zinthu zina ndi kupanga mpweya wa okisijini ndi cakudya . M’malo mwake , makolo adzafunikila kuona zinthu moyenela . 62 : 8 ) Mapemphelo anu angakhale atanthauzo kwambili pamene mupitiliza kum’pempha mocokela pansi pa mtima . Timapindula bwanji tikamaganizila mmene malonjezo a Mulungu adzakwanilitsidwila ? Patapita miyezi ing’ono , mnyamatayo anabatizika pamsonkhano wadela . Inde , panali patangotsala zaka zocepa cabe kuti mzinda wa Yerusalemu uwonongedwe momvetsa cisoni . Tiyeni tione citsanzo ca mlongo wina dzina lake Ana . Nanga bwanji m’Baibulo mukanakhala kuti mulibe mfundo zina zofotokoza cifukwa cake Mulungu anakantha Azariya ndi khate , monga mmene nkhani zina za m’Baibulo zilili ? Ndithudi , Yehova amaona kuti makolo acikhristu ali na mlandu ngati amanyalanyaza udindo wawo wolanga ana moyenelela . ( b ) Nanga zimene taphunzilazo zakukhudzani bwanji ? Panalinso cifukwa cina cimene Mulungu anapelekela malangizo atsopano . Ubwenzi wathu na ena . — Aefeso 4 : 31 , 32 ; 5 : 22 , 25 , 28 , 33 . Komabe , cifukwa cakuti mudzi wathu unali kutali kwambili , sitinakhudzidwe na nkhondoyo . Adamu anali kuyang’anitsitsa nyama iliyonse ndi kuipatsa dzina loyenelela . Ndipo Yehova sanali kuloŵelelapo n’kupelekanso maina ake ayi . Baibulo limaticenjeza mosapita mbali kuti : “ Musasoceletsedwe . N’nali kuopa imfa kwambili . Sinidzaiwala zimene zinacitika tsiku lina madzulo pamene n’nali kubwelela ku nyumba . ( b ) Kodi mau ake onena za masautso a mtsogolo ndi olimbikitsa motani ? 2 : 5 ) Yesu anayelekezela zocitika za pa nthawiyo na zimene tiona masiku ano . Popeza kuti ndinali kukonda kuŵelenga ndi kuphunzila , amai anga anandithandiza kuti ndiyambe kukonda kwambili Yehova , ndipo ndimawayamikila kwambili . Muziŵelenga Baibo tsiku lililonse , ndipo musamanyalanyaze kupemphela . ( Miy . 17 : 17 ) Akhristu afunika kupitiliza kutonthoza mnzawo wofedwa mpaka pamene iye adzakwanitsa kupilila payekha . — Ŵelengani 1 Atesalonika 3 : 7 . PA Pentekosite wa mu 33 C.E . , panacitika cinthu capadela m’mbili ya anthu a Yehova padziko lapansi . Davide anaona kuti ciphona cilibe mphamvu poyelekezela ndi Yehova Mulungu Koma n’zosatheka kudziŵa mmene cosankha cimeneci cingakhudzile banja lanu . ( Miy . MAPINDU AMENE NDAPEZA : Ndinapulumuka cifukwa cophunzila za Yehova . Tingaphunzilepo kanthu pa zolakwa za ena , amene nkhani zawo zinalembedwa m’Mau a Mulungu . ( Zef . 2 : 3 ) Anthu ofatsa amayembekezela Mulungu kuti ndiye adzathetsa zinthu zonse zoipa zimene zicitika ndi mavuto amene akumana nawo . Ku Turkey kuli ofalitsa oposa 2,800 , koma kuli anthu 79 miliyoni . Ndiyeno , yelekezelani zimenezo na zimene wolemba Uthenga Wabwino , Maliko , analemba zoonetsa mmene Yesu anamvelela ataona khamu la anthu . Nthawi zonse , anthu a Yehova amakondwela kusonkhana pamodzi . Atsogoleli acipembedzo Aciyuda , anafuna kuti Yesu akhalebe wakufa m’manda mmenemo kwamuyaya . 1 : 2 , 3 ) Kudekha ndi kukambitsilana naye mwacikondi zingacititse munthuyo kufuna kuphunzila zambili . Conco , anakumbutsa ophunzila ake kuti watsala pang’ono kuphedwa . Anawakumbutsanso kuti onse omutsatila afunika kudzipeleka ndi mtima wonse . Tsiku ndi tsiku , timafunika kusankha zinthu zimene zingakhudze umoyo wathu wa kutsogolo . Koma pali pano , tiyenela kugwila nchito yathu yolalikila mwacangu . Iye amacita cimodzi - modzi kwa ise masiku ano . — Ŵelengani 2 Akorinto 1 : 3 , 4 . Nkhanizo zidzakuthandizani kuganizila Malemba osiyanasiyana mosamala ndi kukulimbikitsani kulemba cifukwa cake mumakhulupilila zimenezo . Nafenso ngati timakonda kuceza ndi anthu amene satumikila Yehova , tikhoza kukumana ndi mavuto . Tikamaŵelenga m’Baibulo mmene Yehova anacilikizila ndi kuphunzitsila anthu ake , timaona kuti Iye amatikondadi . — Ŵelengani Miyambo 3 : 11 , 12 . Makolo , kumbukilani kuti ana anu sanabadwe na khalidwe la kudziletsa . Kodi Mkulu wa Ansembe , Yoswa , anakhala mfumu atavekedwa cisoti cacifumu ? Anthu amenewo akali ndi mwai wopanga cosankha cisautso cacikulu cisanayambe . Nanga n’cifukwa ciani Paulo ndi Baranaba ‘ analimbikitsa ophunzila ’ mwa kuwauza kuti adzakumana ndi masautso ambili ? Paulo analangiza akulu kuti apeleke munthu woipayo kwa Satana — kutanthauza kum’cotsa mumpingo . Ndiponso pamene Luka anali kulemba Buku la Uthenga Wabwino ndi la Machitidwe , anagwilitsila nchito mau oonetsa kuti analidi dokotala . Ngakhale kuti kunali cizunzo ndi mavuto ena , mipingo inaonjezeka m’madela amene tinali kutumikila . Ganizilani citsanzo ca John wa zaka 39 , amene anapezeka ndi khansa yoopsa kwambili . ( b ) Kodi Yesu anacita ciani kudziwelo ? Nanga zimenezi zikutiphunzitsa ciani ? Kambili munthu akalakwa , amathela nthawi yaitali kuimba ena milandu , kapena kulungamitsa zimene zinakambidwa kapena kucitika . A Inoki : Ndaonapo zimenezi . Koma m’zikhalidwe zina olandila alendo amaona kuti ni bwino kuti alendowo asabwele na mphatso iliyonse . Komanso kumatithandiza kuti tisakhumudwe ngati munthu wina amene tinali kum’lemekeza wacita cinacake colakwika . Kodi makolo afunika kuzindikila mfundo iti ngati mwana wawo wobatizika wayamba kufooka m’cikhulupililo ? Nikolai sanali kungocezela mipingo koma analinso kuyang’anila nchito yocita fotokope zofalitsa na kuzitumiza ku mipingo . Kodi zinali “ zinthu za thupi ” ? Njila yabwino yodziyesela ngati tili m’cikhulupililo ndiyo kusinkha - sinkha za anthu okhulupilika a m’Baibulo . Kodi nili ndi pasipoti yovomelezeka ? ( Luka 14 : 8 , 9 ) Mulimonse , kudzikweza kulibe cotulukapo cabwino . Mwamuna ndi mkazi woyamba , Adamu na Hava , atangolengedwa , mngelo wangwilo anaseŵenzetsa molakwa ufulu wake wosankha mwa kuyambitsa cipanduko padziko lapansi . Conco , khulupililani zimene mau ake amakamba pa nkhaniyi , ndipo landilani cikhululuko cake . — Yes . ( Luka 5 : 39 ) Mwina cifukwa sicingakhale cimeneco . Komabe , acinyamata ndiwo ali na mphamvu ndi nyonga kuposa acikulile . ( Miy . ( 1 Samueli 19 : 9 - 11 ; 30 : 1 - 6 ; 2 Samueli 6 : 14 - 22 ) Koma mosasamala kanthu za zinthu zimene anthu anamucita , Davide anali kukondabe Yehova ndi kum’khulupilila . Mungapeze mayankho a mafunso anu pa webusaiti yathu ya www.jw.org . Kodi popanda Baibulo tikanadziŵa bwanji kuti tifunika kuyandikila Mlengi wathu ? 3 , 4 . ( a ) N’cifukwa ciani Akristu satengamo mbali m’mikangano ya m’dzikoli ? Dzina la Yehova limaonetsa bwino - bwino ukulu wake , mphamvu , ndi ciyelo . Kwa Amy , vuto lalikulu linali kuyewa kunyumba . Tisalole ubwenzi wathu na iye kusokonezeka cifukwa ca zocita za ena . William , mnyamata wa zaka 24 , anati : “ Munthu akagwila nchito mwaluso ndi kuona zotsatila zake zabwino , amakhala wosangalala . N’nali kuyesetsa kuwakonda ndi kuwaganizila . Zitsanzo zimene takambilana , ca Marthe ndi ca Henri , zionetsa kuti tingakwanitse kulimbikitsa m’bale kapena mlongo wathu amene afunikila citonthozo . Mwacitsanzo , akulu amafunika kucita zinthu molimba mtima pamene asamalila nkhani zaciweluzo , kapena pothandiza abale na alongo odwala mwakaya - kaya . Mwacitsanzo , mu 1912 , Guglielmo Marconi amene anali mmodzi mwa anthu oyamba kupanga telegalafu , analosela kuti : “ Telegalafu imeneyi idzacititsa kuti nkhondo zithe . ” Ruby , mkazi wa Eduardo anati : “ Ndinafunikila kusenza udindo wa mai ndi tate ndipo ndinazoloŵela kupanga zosankha m’banja . Kodi inu mukanacita bwanji ? Sitingathe kudziŵa tsiku lenileni pamene zinthu zoipa ndi kuvutika zidzatha . Yesu anati : “ Kunena za tsikulo ndi ola lake , palibe amene akudziŵa , ngakhale angelo akumwamba kapenanso Mwana , koma Atate yekha . ” Nanga mumamva bwanji ponena za ciyembekezo cimeneci ? Pamene Yesu anacita cozizwitsa cake coyamba , cimene ndi kusandutsa madzi kukhala vinyo , Yosefe sachulidwako . Iye sachulidwakonso ngakhale pa zocitika zina za pambuyo pake . Citsanzo cao cimakumbutsa Mkristu aliyense kuti cimakhala cinthu canzelu “ kusangalala ndi amene akusangalala . ” — Aroma 12 : 15 . Tingatengele bwanji citsanzo ca Nowa ? A Zimba : Hmm . Mokoma mtima , iye ananifotokozela mbali zimene n’nafunika kuwongolela , komanso maluso amene woyang’anila dela wabwino amafunika kukhala nawo . Nanga n’cifukwa ciani tikukamba kuti fanizoli limagogomezela kufunika kolalikila ? Yesu anali kuuza ophunzila ake mobwelezabweleza kuti anali kuwakonda . N’zocititsa cidwi kuti mu 2011 , Bungwe Lolamulila linasintha nthawi imene atumiki a pa Beteli ku United States anali kuyamba kucita Phunzilo la Nsanja ya Mlonda , kucoka pa 18 : 45hrs kubwela pa 18 : 15hrs . ( Nyimbo 2 : 7 ; 3 : 5 ) N’cifukwa ciani anatelo ? Nanga tingaonetse bwanji kuti ndise alendo abwino ? Iye watilola kudzisankhila kaya kumumvela kapena ai . Nthawi zina , Mkhristu angapemphedwe kuti aziphunzitsa Baibo ana amene makolo awo sali m’coonadi . 25 : 31 - 33 ) Pambuyo pake , sikudzakhalanso mabungwe acinyengo . N’nakhudzidwa mtima na zinthu zambili zimene n’naphunzila m’Baibo . Tingakondwele ngako na coonadi ca m’Baibo cimene taphunzila , koma abululu athu angaganize kuti tapusitsidwa kapena taloŵa m’kagulu kampatuko . Koma pamene mukukula mwauzimu , mumadzionela mwekha dzanja la Yehova mu umoyo wanu . ( b ) Kodi tidzakambilana mafunso ofunika ati okhudza kukhala munthu wauzimu ? Pamene M’bale Hughes anayamba kupeleka zifukwa zodzikhululukila , M’bale Rutherford anamudzudzula mwamphamvu . Mofananamo , m’bale wobatizika akhoza kukhala wolimba mtima ngati apempha thandizo kwa Mulungu mwa kupemphela mocokela pansi pa mtima ndi kuŵelenga Baibo tsiku na tsiku . Kodi muganiza kuti n’cifukwa ciani Yesu anadziŵitsa dzina la Mulungu ? Sara akanakamba kuti Abulahamu ni mwamuna wake , Abulahamu akanaphedwa . Patangopita nthawi yocepa , amai anga a Estelle anayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . Koma zimenezi si zoona cifukwa makhalidwe abwino amenewa ni ocokela kwa Yehova , amene ni wamphamvu kwambili kuposa aliyense m’cilengedwe . Koma mnyamatayo amene anathandiza anakambilana ndi anzake a mumzinda wina wotsatila umene basi imaimilila . Iye anabweza nkhongoleyo yokwana madola 20 . Nkhani yakuti “ Mafunso Ocekela kwa Aŵelengi ” mu Nsanja ya Mlonda ya November 15 , 2014 , inafotokoza za kusintha kaikidwe ka akulu na atumiki othandiza paudindo . Monga mmene timaseŵenzetsela galasi kuti tione maonekedwe athu , tifunika kugwilitsila nchito Baibulo kuti tione mmene umunthu wathu wamkati ulili ndi kukonza zolakwika zilizonse . Mphamvu zimandithela ndikayamba kuganizila mmene mkazi wanga anavutikila ndi kansa . ” Ngati tikhululukila ena timaonetsa kuti timakhulupilila Yehova . Ndinamupanga kukhala coseketsa kwa onse a m’dela lathu . Conco , mu 1982 , tinakwatilana . GANIZILANI ZITSANZO ZOCEPA IZI . Yehova atapulumutsa Aisraeli mu ukapolo ku Iguputo , anawapatsa malamulo . Malamulowo anaonetsa kuti iye anali kuganizila anthu amene sanali Aisraeli , omwe anayamba kulambila koona . ( Eks . “ Yehova amayang’anila alendo okhala m’dziko la eni . ” — SAL . 5 : 10 ) Baibulo limakamba kuti mitu ya banja ili ndi udindo m’banja . Conco , mutu wa banja ungaone zosangulutsa zosayenelela banja lake . Tonse timafunikila cilimbikitso , maka - maka pamene tikukula . Ganizilani cisangalalo cimene Rabeka anali naco mumtima , atazindikila kuti lonjezo la Yehova lidzakwanilitsidwa kudzela mwa Isaki , amene anali kudzakhala mwamuna wake , ndiponso mwa iye . — Genesis 22 : 15 - 18 . [ Zinenelo 36 ] 14 : 21 ) Mulimonsemo , cimene tidziŵa n’cakuti mtundu wonse unatsatila zocita zake . ( 1 Tim . 4 : 16 ) Kaya anthu amve uthenga wathu kapena akane , tidzadziŵa kuti tacita zimene tingathe kuti tikwanilitse ulaliki wathu . ( 2 Tim . Inu akulu , Yehova amafuna kuti muzicitila cifundo nkhosa zake . Iye anadziŵa kuti mwana amene anapezayo anali wa Aheberi ndi kuti anafunika kuphedwa . Caciŵili , angelo anathandiza bungwe lolamulila . Ngati inunso mufuna kugwila nao nchitoyi , ganizilani nkhaniyi mwapemphelo . Ngati zinalidi conco , kodi otsatila ake anafunika kucita ciani ? Pa nthawi ina , tinali kuoloka mtsinje pa bwato . Bokosi limene lili m’nkhani ino lionetsa zocitika zosiyanasiyana zimene Baibulo limakamba . Mtumwi Paulo anakamba kuti : “ Mulungu amacita zinthu m’njila imene imamusangalatsa . Iye amalimbitsa zolakalaka zanu kuti mucite zinthu zonse zimene iye amakonda . Panthawi imeneyi , kukhulupilika kwathu kwa Mulungu kumayesedwa . Ca m’ma 1941 tinazindikila kuti Akhiristu sayenela kugwila nchito pa kampani yokonza zida za nkhondo . ( Sal . 1 : 2 , 3 ) Pamene tisinkhasinkha uthenga wa m’Baibo , mzimu wa Mulungu umatithandiza kumvetsetsa mmene Yehova amaonela zinthu pa nkhani zosiyana - siyana . Yehova sanam’siye Yosefe , na imwe sadzakusiyani ( Onani palagilafu 13 ) Ganizilani njila zosiyanasiyana zolalikilila zimene mungakwanitse kucita . Kuti mudziŵe zimene timakhulupilila , cifukwa cake sitikondwelela maholide , ndi cifukwa cimene sitilolela kuikidwa magazi , pitani pa www.jw.org polemba kuti ZOKHUDZA IFE > MAFUNSO OFUNSIDWA KAŴILIKAŴILI . MBALI imodzi ya cizindikilo ca “ mapeto a nthawi ino ” cimene Yesu anakamba ni yakuti , “ cikondi ca anthu ambili cidzazilala . ” ( Mat . Ndipo vuto lalikulu n’lakuti tingapangitse kuti ayambe kudzikweza . Podziŵa zimenezi , Yehova anauza Mose kuti amulimbikitse Yoswa . mu Galamukani ! ya August 8 , 1995 . Kodi kholo lingathetse bwanji vutoli ? 10 : 16 ) Naonso amatumikila Khiristu , ndipo akucita mbali yaikulu pa nchito yolalikila . Akuphunzitsa anthu coonadi ndi kuwathandiza kukhala pa ubwenzi ndi Yehova . Maphunzilowo angaphatikizepo kuthandiza wofalitsa watsopano ( 1 ) kukonzekela ndi kuyeseza ulaliki , ( 2 ) kuloŵetsa mwininyumba kapena munthu amene akumana naye pamseu mumakambilano , ( 3 ) kugaŵila zofalitsa , ( 4 ) kupanga ulendo wobwelelamo kwa munthu wacidwi , ndi ( 5 ) kuyambitsa phunzilo la Baibulo . Kodi atsogoleli acipembedzo anacita ciani ? Pangano la Davide linapeleka malangizo oonjezeleka ponena za mzele wobadwila wa Mesiya . Pangano limenelo linacititsanso Yesu kukhala ndi mphamvu zolamulila padziko lapansi kwamuyaya . Musamadzidalile . Nchito Yofalitsa Mabuku . 16 : 24 ) Inde , kukhala wophunzila wa Yesu , kumene kumaphatikizapo kudzipeleka na kubatizika , n’kofunika kwa Mkhristu aliyense . SALIMO 104 : 24 , 25 Kodi tikuphunzilapo ciani pamenepa ? Cinthu cina cosangalatsa paumoyo wanga cinali kupatsidwa mwai wokapezeka pa msonkhano wacigawo ku Tuvalu mu 2011 . Popeza kuti tsiku la Yehova layandikila , Paulo anatilangiza kuti , “ tiganizilane kuti tilimbikitsane pa cikondi ndi nchito zabwino . ” ( Aheb . Yesu anakamba kuti ‘ amabadwanso . ’ Anthu atayamba kuŵelenga Baibo anayamba kufunsa kuti : ‘ Kodi pegatoli yowochelako mizimu ya anthu ocimwa inalembewa pati ? Manda akupitiliza kutenga anthu , ndipo siyapeleka ciyembekezo ciliconse . Anthu amafuna kukhala na umoyo waphindu , wacimwemwe ndi wotetezeka . Conco , pamene muŵelenga Baibo , muzimupempha kuti akuthandizeni kuimvetsetsa , kukumbukila mfundo zimene mwaŵelenga , na kuziseŵenzetsa mu umoyo wanu . — Ezara 7 : 10 . Mofanana ndi anthu a ku Europe , anthu a ku France samapemphela kuti alambile Mulungu . Analinso kuganizila ngati n’kwanzelu kusamukila mumzinda wa New York , ndiponso ngati mwana wao angazoloŵele umoyo watsopano . Koma Mulungu angathandize ena kucita nchitoyo . — Sal . Kaŵili - kaŵili anthu amene amakonda kucitila ena cifundo , nawonso amathandizidwa pamene afunikila thandizo . — Ŵelengani Mateyu 5 : 7 ; Luka 6 : 38 . Komabe , sizinanivute kujaila umoyo watsopano cifukwa n’nali kusangalala na maphunzilo a Giliyadi . Cifukwa ca zimene zinamucitikila m’mbuyomo , mlongo wina anali kuona kuti n’zovuta kukonda Yehova . Alinso na mphamvu zoukitsa akufa ndi kuthetsa masoka a zacilengedwe . Tinazindikila kuti monga Akhristu obatizika , tifunika kulalikila nthawi zonse potsatila citsanzo ca Yesu . Kumatithandiza “ kukana moyo wosaopa Mulungu ndi zilakolako za dziko , koma kukhala amaganizo abwino , acilungamo ndi odzipeleka kwa Mulungu m’nthawi ino . ” — Tito 2 : 12 . Mungadzifunse kuti , ‘ Kodi ana anga amakonda utumiki cifukwa cakuti amangofuna kuti tiime pamalo ena ake ndi kuwagulila cakudya kapena zakumwa zozizilitsa kukhosi ? ’ ( Ŵelengani Miyambo 22 : 7 . ) ( Yobu 38 : 4 , 7 ) Kuyambila kale , angelo akhala akulaka - laka ‘ kusuzumila ’ m’maulosi okhudza zocitika za kutsogolo padziko lapansi . — 1 Petulo 1 : 11 , 12 . ( 1 Yohane 3 : 16 ) Komabe , popeza nsembe imeneyo inali mbali ya colinga ca Mulungu , nkhani zino zotsatizana zidzafotokoza kwambili udindo wa Mulungu monga Wopeleka dipo . Baibulo si buku la nthano . Umboni wa sayansi waposacedwapa waonetsa kuti cilengedwe cikukulilakulilabe ndipo zimenezi zikucitika mofulumila kwambili . Kumbukilani kuti Yesu anati : “ M’masiku amenewo cigumula cisanafike , anthu anali kudya ndi kumwa . Nili na amuna anga , a Bright , pamene tinali kutumikila monga amishonale ku Asunción , m’dziko la Paraguay Ngati timatangwanika ndi nchito ya Yehova , tidzapewa kudela nkhawa za mavuto athu nthawi zonse Atumiki ena a Mulungu alankhulapo mau ngati amenewa pankhani yopeza munthu wokwatilana naye . “ Anatsegulilatu maganizo ao kuti amvetse tanthauzo la Malemba . ” — LUKA 24 : 45 . ( Ŵelengani Yesaya 11 : 9 . ) Anawatsimikizila kuti Yehova sadzalola kuti kulambila koyela kuipitsidwe . ( 2 Tim . 2 : 19 ) Iye amaona ciliconse cimene timacita na kukamba . ( Aheb . Cifukwa ca cifundo , Yesu anali kulankhula ndi ena mokoma mtima makamaka ovutika . Kuwonjezela apo , ngati timakhutulila Yehova zakukhosi m’pemphelo , timam’yandikila . Koma masiku ano , timaicha nkhondo yoyamba ya padziko lonse . Koma ena asankha zosiyana ndi zimenezi . ( Chiv . 17 : 17 ) Mapeto adongosolo lino sali patali . Ngati ticita zimenezi , ifenso tidzakhala na umoyo wopambana , komanso tidzacita zinthu mwanzelu . ( 1 Yohane 5 : 19 ) Pambuyo pakuti Yehova waononga Satana ndi ziwanda zake , ndiponso dziko loipali , anthu padziko lonse adzakhala okondana . Ngati wina wanilakwila , kodi nimakhala wofunitsitsa kukambilana naye kuti nibwezeletse mtendele ? ’ Ndiyeno , sankhani lemba loyenelela . ( Ŵelengani 1 Petulo 3 : 3 , 4 ; Yer . Mwacionekele , anali kuopa kuti Farao sadzam’landila ndi kumumvela monga woimilako Yehova Mulungu . Kodi Zinacitikadi ? Tinasankha zogwilitsila nchito njila imene anthu ambili amaona kuti ndi yabwino pophunzila cinenelo catsopano . Mtumwi Petulo analemba kalata yolimbikitsa Akristu kuti apilile ziyeso zocokela kwa Satana zimene anali kukumana nazo . Iye analemba kuti : “ Khalani olimba m’cikhulupililo ndipo mulimbane naye , podziŵa kuti anzanunso m’gulu lonse la abale anu m’dzikoli akukumana ndi masautso ngati omwewo . ” 1 : 21 . 4 : 29 ) Aliyense wa ise ayenela kukhala chelu kuti adziŵe zimene ena ‘ akufunikila . ’ Ulendowo uyenela kuti unali wovuta kwambili pa maulendo onse a Abulahamu . Conco , n’kutheka kuti Yesu anapita ku Yerusalemu ngakhale kuti zimenezo zikanamutengela nthawi yaitali . Kodi mumaona Yehova monga Tate wacikondi ndi Bwenzi lapamtima ? Kodi mumakhulupilila kuti adzakuthandizani pamene mwakumana ndi mavuto ? Koma kodi zonsezi zikukhudza bwanji Ufumu wa Mulungu ndi caka ca 1914 ? Iwo acititsa anthu ambili kuona kuti kukhulupilila kuti kuli Mlengi ni umbuli ndiponso n’kupanda nzelu . ‘ Mau a pakamwa panga . . . akukondweletseni , inu Yehova . ’ — SALIMO 19 : 14 . Kudzicepetsa kumatithandiza kulemekeza ena ndi kuwacilikiza . — Aroma 12 : 10 . Ngati wina wakukhumudwitsani , mungacite bwino coyamba kutsatila malangizo a m’Baibo a pa Akolose 3 : 12 - 14 . Timayamikila kwambili Yehova kaamba ka kukoma mtima kwake kwakukulu . Motelo , tiyenela kuseŵenzetsa mphamvu zathu pomutamanda ndi kuthandiza ena . Kuti mudziŵe zambili , onani nkhani yakuti , “ Kulambila kwa Pabanja N’kofunika Kwambili Kuti Tidzapulumuke ” mu Nsanja ya Olonda ya October 15 , 2009 , masamba 29 - 31 . M’Baibulo , Mfumu Azariya imachedwanso Mfumu Uziya . Conco , m’nkhani ino tikambilana mafunso awa : Kodi Yehova watithandiza bwanji kumvetsa fanizo limeneli ? 3 : 3 , 4 ) Kodi n’ciani cimene cimapangitsa anthu ena kuganiza conco ? Iwo saphunzitsa zakuti Ufumu wa Mulungu udzathetsa mavuto onse a anthu ndi kuti posacedwapa udzacotsa zoipa zonse padziko lapansi . YANKHO : Mzimu woyela ni mphamvu imene Mulungu amaseŵenzetsa pokwanilitsa cifunilo cake . 32 : 4 . Tattannu ndiye Tatenai wochulidwa m’buku ya m’Baibo ya Ezara . Katswili wina wa zamaganizo a ana , anakamba kuti zaka za unyamata zimakhala zovuta kwa ana ndi makolo . Fanizolo linamukhudza mtima Davide cifukwa iye anali m’busa panthawi ina . N’kulakwa kuyamba kukaikila abale ndi alongo athu popanda maziko enieni . ( Miy . 2 : 1 - 5 , 10 , 11 ) Tingaphunzilenso za Yesu ndi kutengela citsanzo cake cabwino pankhani yokhala wozindikila . Koma mu 1942 , pamene Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse inali mkati , M’bale Nathan Knorr yemwe anali kutsogolela Mboni za Yehova , anakamba nkhani pa msonkhano wacigawo ya mutu wakuti “ Kodi Padzikoli Padzakhala Mtendele ? ” Cifukwa cokonda Mulungu ndi kum’tumikila , anthu a Yehova anafulatila nchito zawo zakale asanadziŵe Mulungu . Mose anali paubwenzi wathithithi ndi Yehova . Yehova anam’gwilitsila nchito cakuti Baibulo limanena kuti Mulungu anali kum’dziŵa “ pamasom’pamaso . ” ( Deut . Mwacitsanzo , akelubi a golide amene anali pamwamba pa likasa la pangano anapangidwa mwaluso kwambili . Koma “ zinthu zimene timalakalaka ” ni zinthu zimene timafuna kukhala nazo , koma n’zosafunika kwenikweni kuti munthu akhale na moyo . ( Mac . 18 : 2 , 3 ) Mwina mungafunike kucitako kosi yaifupi kuti mudzathe kupeza nchito ya maola ocepa m’dela lanu . Muganiza kuti Yehova amamvela bwanji akaona kuti mukucita zimene mungathe kuti muyandikile iye ndi Mwana wake ? Ngati mumakhulupilila kuti Yehova adzakutetezani pa ‘ tsiku lake lalikulu ndi locititsa mantha , ’ mudzatha “ kuona cipulumutso ca Yehova , ” ndipo mudzakhala olimba . — Yow . 2 : 31 , 32 . NYIMBO : 104 , 152 Ndiye cifukwa cake , pamene Paulo anali kuphunzitsa Timoteyo , anam’limbikitsa kuti ‘ azifotokoza bwino mau a coonadi . ’ ( 2 Tim . Ngati thandizo limapelekedwa kwa makolo nthawi ndi nthawi , makolo sangafunikile kupita kukakhala kunyumba yosungila okalamba . ( Yobu 1 : 9 - 12 ) Ndipo ndi Satana yemweyo amene anayesa Yesu . Baibulo limagwilitsila nchito mau akuti “ maziko , ” kunena zinthu zosiyanasiyana . Mwacitsanzo , Yerusalemu mzinda waukulu wa Isiraeli umanenedwa kuti maziko . Ndipo anthu mamiliyoni ambili amene ali ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha padziko lapansi akulengeza nao uthenga umenewo . Iwo anali kuchula makalavani amenewo kuti Yehu , potengela dzina la Yehu , woyendetsa galeta amene anadzakhala mfumu mu Isiraeli . Njila imodzi imene Mulungu amatithandizila kulimbana ndi mavuto , ni kupitila m’pemphelo . Ngati mufuna kuonjezela utumiki wanu mwa kutumikila ku malo kumene kufunika ofalitsa ambili a Ufumu , musakaikile kuti mudzapeza madalitso osaneneka . Yehova naye amathandiza Akhiristu kulimbana ndi nkhawa pamisonkhano ya mpingo ya mlungu na mlungu . Mikangano ina ingafunike kuti ena athandizileko malinga ndi zimene lemba la Mateyu 18 : 15 - 17 limakamba . Mosiyana ndi tsunami , zivomezi kapena kuphulika kwa mapili , nkhondo imene ikubwela sidzapha anthu osalakwa . Ena amaona kuti cofunika ngako ni banja lawo , thanzi , kapena zinthu zina zimene afuna kucita paumoyo . Zaciwawa zimacitikila anthu osalakwa . Kodi cenjezo la Paulo pa Aroma 8 : 6 sililetsa ciani ? Chimo limene Yesu anakamba lingaphatikizepo zinthu monga cinyengo kapena misece . Koma siliphatikizapo macimo monga dama , kugonana kwa amuna kapena akazi okhaokha , mpatuko , kapena kulambila mafano . M’zaka 100 zoyambilila , magulu aŵili ochuka aciyuda , Aesene ndi Afarisi , anali kuphunzitsa kuti munthu akafa , mzimu wake umapitiliza kukhala na moyo . Tifunika kukhala osamala kuti tipewe kulemekeza anthu ena mopambanitsa . Ndipo khalani ndi cidalilo cakuti Yehova adzakuthandizani kukhala olimba kuuzimu . — Sal . Mulungu polenga munthu woyamba , Adamu , anam’patsa mphatso ya ufulu wosankha zocita imenenso anapatsa angelo kumwamba . Nkhanizi zidzafotokoza zocitika zitatu za m’Baibo , zimene zidzatithandiza kucita zinthu mogwilizana ndi cilungamo ca Yehova . Yesu analimbikitsa otsatila ake kuti : “ Onetsani kuwala kwanu pamaso pa anthu , kuti aone nchito zanu zabwino ndi kuti alemekeze Atate wanu wakumwamba . ” — Mateyu 5 : 16 . N’cifukwa ciani makolo ena acikhristu amalimbikitsa ana awo kuti asabatizike mwamsanga ? Kodi zimenezi zinacititsa ophunzila ake kuyamba kumupeputsa ? Mitsinjeyo ikuganizilidwa kuti ikuimila kufalikila kwa Cikhristu ku mbali zinayi za dziko lapansi . Satana anali kudana kwambili ndi anthu a mu mzele wobadwila wa Mesiya . Zikakhala conco , makolo awo safunika kuona ngati kuti anawo akuwakana . ( 1 Yohane 4 : 9 ) Kodi unali udindo wa Mulungu kucita zimenezi ? Zimenezi zinayamba kucitika kutatsala zaka mahandeledi ocepa kuti masiku otsiliza ayambe . Mwacitsanzo , yelekezelani kuti muli pamzela wogaitsa cimanga kucigayo . Usamaope kapena kucita manyazi kupempha thandizo langa . Mwacitsanzo , amishonale akasamukila ku dziko lina , zinthu kumeneko zimakhala zosiyana ndi za kwao ndipo amafunika kucita khama kuti azoloŵele umoyo watsopano . 3 : 1 - 17 ) Mwacidziŵikile , kuwonjezela pa Yesu , Yohane M’batizi yekha ndiye anamvako mau amenewa . Ganizilani mmene Rabeka akanamvelela , akanamva nkhani imene Eliezere anafotokozela acibale ake . Kodi anthu a Mulungu analoŵa bwanji mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu kuyambila m’ma 100 C.E . kupita m’tsogolo ? ( Yohane 16 : 12 ) Naonso abale a ku Japan anayembekeza nthawi yabwino youza anthu za ciukililo . Kodi zimenezi zikutanthauza kuti anthu amenewa sanali okhulupilika kwambili kapena sanali oyenelela kukalamulila kumwamba ? Cotelo , kodi Baibulo limanena kuti anthu amene anafa asanadziŵe Mulungu ali ndi ciyembekezo cotani ? Koma panali vuto . Ndipo watiuza zifukwa zimene tiyenela kucitila zimenezi . Mofananamo , pamene Yesu anatiitana kuti tim’tsatile , tinadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa . Nanga unasiyana bwanji ndi nthawi ina iliyonse m’mbili ya anthu ? M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene tingagwilitsile nchito bwino mphatso yathu yocokela kwa Mulungu yotha kuganizila zamtsogolo . ( Mat . 4 : 4 ) Ndipo anakhalabe womvela Mau a Mulungu mpaka kufa pa mtengo wonzuzikilapo . “ Mwana wanga wamkazi analila mogonthetsa m’kutu , cakuti ndinada nkhawa kwambili . Anayambanso kudandaula za cakudya cimene Yehova anali kuwapatsa , mpaka anafuna kubwelela ku Iguputo . Kaya takhala nthawi yaitali motani m’coonadi , timadziŵa kuti mavuto ndi osapeweka m’dziko la Satanali . — Chiv . Kumacititsa munthu kukhala na thanzi labwino , maganizo abwino , komanso kudzimva kuti ali pa ubwenzi wabwino na Mulungu Atautsa mutu wake pa pilo kuti adzuke , kunatuluka njoka imene inabweletsa mkosokonezo kufikila n’taipha . Pamene Aisiraeli anali m’Iguputo , anali osauka ndi ofooka . Conco , asanaloŵe m’Dziko Lolonjezedwa , anauzidwa kuti sadzafunika ‘ kuumila mtima ’ abale ao ovutika . Anthu ambili ndi osakonda acibale , oopsa , ndi osakonda zabwino . ( 2 Tim . Kuti Munthu Akhale Mtumiki , Kodi Afunika Kukhala Wosakwatila ? Tifunika kusamala kwambili maka - maka tikamakamba za abale amene ali paudindo mumpingo . — Ŵelengani Aheberi 13 : 17 ; Yuda 8 . Lembali linena kuti : “ Ine ndacititsa kuti io adziŵe dzina lanu ndipo ndidzapitiliza kuwadziŵitsa dzinalo kuti cikondi cimene munandikonda naco cikhale mwa io , inenso ndikhale wogwilizana ndi io . ” Katie anayankha kuti , “ Inde a Robby , ndipo mtsikana amene wakupatsani foniyo ndi mkulu wanga . Kodi mufuna kutengela Yosiya m’njila ziti ? Aliyense abwelele kunyumba kwake , cifukwa zimene zacitikazi , zacitika mwa kufuna kwanga . ” — 1 Maf . ( Yelekezelani ndi Yakobo 1 : 14 , 15 . ) ‘ Tsopano Ndinu Anthu a Mulungu , ’ 11 / 15 M’Baibo , kuyenda na Yehova kumatanthauza kum’dalila , kucilikiza ucifumu wake , na kutsatila citsogozo cake . Kodi makhalidwe oipa amatikhudza bwanji masiku ano ? Ndi udindo wotani umene tili nao wopezeka pa Salimo 48 : 12 - 14 ? Pa msonkhanopo , panapezeka anthu 50 . N’nacita cidwi kuona kuti ngakhale ana acicepele anali kupeleka ndemanga pa nkhani zozama za m’Baibo . Kodi cikhulupililo canga cimanilimbikitsa kutsatila mfundo zolungama za Mulungu na kuphunzitsakonso ena mfundozo ? ’ Zikanakhala kuti Adamu na mbadwa zake za m’tsogolo anamvela lamulo la Mulungu , sembe iwo sanacimwe na kulaŵa imfa . Mwacionekele , nthawi zambili iye anali kukumbukila mmene zinthu zinalili pamene anali kupita ku mapili a ku Hebroni kukadyetsa nkhosa za atate ake . ( 1 Maf . 2 : 3 ) Komabe , Malemba aonetsa kuti Yehova ndiye anapeleka Cilamulo , ndipo Mose anali pansi pa Cilamuloco . Iye anapeleka ndalama zomangila kacisi ndi kulimbikitsa anthu kuti acilikize nchitoyo . Ndi zitsanzo ziti zimene zionetsa kuti Yesu anali wosakwiya msanga ndi woganizila ena ? Kodi akufa adzauka liti maka - maka ? ’ 20 : 28 ) Nthawi zonse Yehova amatifunila zabwino . Conco , iye watipatsa akulu mumpingo . Atsikana athu anatiuza kuti citsanzo cimene ise ndi ambuye awo tinawaonetsa cinawathandiza kumvela lamulo la Yesu lakuti , “ pitilizani kufuna - funa Ufumu coyamba , ” ngakhale pamene akumana na vuto la ndalama . ( Mat . Mavuto ena angacitike mwadzidzidzi , koma ena angatenge nthawi yaitali . 24 : 15 ) Ndithudi , tidzasangalala kwambili kulandila akufa amene adzaukitsidwa ndi kuwaona akusangalalanso ndi moyo . Mulungu “ adzapukuta misozi yonse m’maso mwawo , ndipo imfa sidzakhalaponso . Ulaliki wapoyela ni njila imodzi yabwino kwambili yoyalikilila . Kale , zofalitsa zathu zinali kufotokoza kuti munthu aliyense , cocitika ciliconse , ndi cinthu ciliconse m’nkhani zopezeka m’Baibulo , zinali kuimila winawake kapena cinacake . Nanga tikapanga cosankha , ndiye kuti sitingacisinthe zivute zitani ? Kodi tingatengele bwanji citsanzo ca Khristu aliyense payekha ? Posacedwapa , anthu amene amakana kuvomeleza ulamulilo wa Yesu Kristu , yemwe ndi Wokwela pahatchi yoyela , adzakakamizika kuvomeleza kuti analakwitsa zinthu kwambili . Ndipo ngati mwalephela kupeleka mphatso yabwino “ koposa , ” mungacite ciani kuti mphatso imene mwapeleka iyamikilidwe ? Magazini ino ya Nsanja ya Mlonda , ifotokoza cifukwa cake Mulungu anatuma Yesu padziko lapansi kuti adzatifele . Ponena za wosauka , Baibulo limatiuza kuti Mulungu “ adzalanditsa wosauka wofuulila thandizo . ” NKHANI YA PACIKUTO | ZIMENE MULUNGU WAKUCITILANI ( 1 Timoteyo 6 : 7 , 8 ) Anthu amene ni okhutila , nthawi zambili sadandaula ndipo zimenezi zimawathandiza kupewa kaduka . “ Ngale imodzi yamtengo wapatali ” imaimila coonadi ca Ufumu camtengo wapatali . Ena amadwala - dwala , ena amasamalila makolo ao okalamba kapena ana amasiye . 18 , 19 . ( a ) Yehova anakambilatu ciani ponena za mtundu watsopano ? Lelolino anthu akupanga zida zankhondo zotsogola kwambili zimene zikuwacititsa kukhala ndi mphamvu zoononga dziko . Pamene Satana anayesa Yesu kuti asandutse miyala kukhala mikate , Yesu anayankha kuti : “ Munthu sangakhale ndi moyo ndi cakudya cokha , koma ndi mau onse otuluka pakamwa pa Yehova . ” ( Mat . Russell anam’khudzila . Kodi malifalensi aŵili amenewa akugwilizana motani ? Mu February 1971 , pa Sondo , ndinapita ku Nyumba ya Ufumu ya Mboni za Yehova ku Delray Beach , ku Florida . 4 : 7 ; 1 Pet . 5 : 9 ) Koma Satana amakondanso kuukila anthu acicepele . Davide anali kuika mwala m’kathumba ka gulaye n’kuzungulutsa gulayeyo mwamsanga pamwamba pa mutu wake , kenako n’kuponya mwalawo mwamphamvu mwa kutaya nthambo imodzi . Yehova anapatsa Nowa mapulani ndi malangizo a kamangidwe ka cingalawa cacikulu kuti iye ndi anthu a m’banja lake adzapulumukilemo . Kodi cidziŵitso cimene muli naco mungacigwilitsile nchito bwanji mokwanila ? 3 Anadzipeleka na Mtima Wonse Zokolola za pa famu tinali kuzikonza ndi kuzisungila pa famu pomwepo . Iwo akapemphedwa kukatumikila kumalo osoŵa , amakamba kuti : “ Ine ndilipo ! Khalani odzicepetsa : Popemphela pamodzi ndi ana anu , io aziona kuti mukupempha Yehova kuti akuthandizeni . ( Yohane 2 : 2 , 6 - 10 ) Iye analinso kupita kukaceza kunyumba za mabwenzi ake , ndi kwa ena amene anali kucita cidwi ndi uthenga wabwino . Iwo adzatithandiza ‘ kukhala olimba m’cikhulupililo ’ pamene tikukhala m’nthawi yovutayi . ( 1 Akor . 16 : 13 ; Miy . Kodi Yesu anayankha bwanji atayesedwa ndi Satana ? Ndipo citsanzo cimeneco cikutiphunzitsa ciani ? Nanga bwanji za makampani adyela amene amawononga cilengedwe ndi kudyela masuku pamutu makasitomala awo , pofuna kuunjikila cuma anthu oŵelengeka pamene anthu mamiliyoni ambili akuvutika ndi umphaŵi ? Koma Baibo imati : “ Atangokhala wamphamvu , mtima wake unadzikuza mpaka kufika pom’pweteketsa . Katswili wolemba mbili ya Ayuda , Josephus , anafotokoza kuti Yudasi “ anali kusonkhezela anthu kuukila boma , mwa kuwanena kuti ni amantha cifukwa cololela kupeleka msonkho kwa Aroma . ” Mulungu wokhulupilika , amene sacita cosalungama . Iye ndi wolungama ndi woongoka . ” Baibo imati : “ Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha . ” — Yohane 3 : 16 . Iye anati : “ Mau a pakamwa panga ndi kusinkhasinkha kwa mtima wanga , zikukondweletseni , inu Yehova , Thanthwe langa ndi Wondiombola . ” — Salimo 19 : 1 , 7 , 14 . Kodi Mkhristu angapilile bwanji imfa ya munthu amene anali kum’konda ? Tili ndi zifukwa zomveka zoyembekezela malonjezo a m’Baibulo . Akazi ena okhulupilika Izi zinakumbutsa Sara kuti wakhala umoyo wokuka - kuka kwa zaka zambili . Ngakhale anthu amene akuyesetsa kukondweletsa Mulungu masiku ano , amakhala ndi nkhawa . ( Yoswa 6 : 17 , 18 ) Limakambanso kuti Aisilaeli anaononga mzinda wa Yeriko m’nyengo yokolola , nthawi imene mumzindawo munali zakudya zambili . ( Ŵelengani Miyambo 29 : 25 . ) ( Aroma 8 : 22 ) Kunena zoona , tifunika dziko latsopano mmene Mulungu adzathetselatu matenda onse monga mmene analonjezela . Mumaona bwanji ngati mukambilana ndi ena ? Mphatikila ya kumbuyo ndi ya kutsogolo anailemba m’zilembo zanthawi zonse ( zosada kwambili ) . Patapita zaka 5 , mu 1535 , womasulila wina wa ku France , dzina lake Olivétan , anatulutsa Baibo imene anaimasulila kucokela ku zinenelo zoyambilila . Baibo imakamba momveka bwino pankhaniyi kuti : “ Abambo , . . . muwalele [ ana anu ] m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake . ” M’Baibulo muli zitsanzo zambili za atumiki a Mulungu okhulupilika amene analandila mzimu woyela wa Yehova , koma sanapite kumwamba . Timakhulupilila kuti Mulungu angacite ciliconse cofunikila kuti atithandize kucita cifunilo cake . ( 2 Akor . Ni lonjezo lofunika kwambili liti limene Mkhristu angapange ? Kunena zoona , zocitika zimene zinalembedwa pa Salimo 45 zimakhudza Akristu onse . Kodi tonsefe timafanana bwanji ? Iye ‘ anapita kukagonjetsa adani ake ndipo anapambana pa nkhondo yolimbana nao . ’ 1 : 11 ) Mulungu anayankha pemphelo la Hana , ndipo iye anabeleka mwana woyamba wamwamuna . Conco , kuti tidziŵe zimene Yehova amafuna , tiyenela kudalila thandizo limene watipatsa . Pa nthawi ina , Mulungu , amene amasanthula mitima analola Hezekiya kuonetsa zimene zinali mumtima mwake . Komanso bwanji ngati m’bale amene anakulakwilani akupitiliza kutumikila monga mkulu kapena akulandila maudindo ena owonjezeleka , kodi mudzakondwela naye limodzi ? Tili kumeneko , ana athu aamuna , Yaroslav ndi Pavel , anabadwa . Yakobo , amene anali m’bale wake wa Yesu , anauzilidwa kulemba kuti : “ Lezani mtima abale , kufikila kukhalapo kwa Ambuye . ” ( Yak . Tikamamvela Yehova monga Wolamulila wathu , timaonetsa kuti iye ndi woyenela kutiuza zimene tiyenela kucita . — Miy . Zimene anacitazo ndi “ citsanzo ca zinthu zimene zidzacitikile anthu osaopa Mulungu m’tsogolo . ” 9 : 17 - 27 ; 10 : 1 . Koma matanthwe a ku Meriba waciŵili ni ofooka . Posacedwapa , magulu andale m’dziko la Satanali adzagwilizana kuti awononge anthu a Mulungu . ( Ezek . 38 : 2 , 10 - 12 ; Dan . ( 1 Petulo 3 : 1 - 5 ) Kukongola kwa conco n’kumene ife tonse tifunikila kukhala nako . 35 : 33 , 34 . Pamene mukumvetsela kalatayo ikuŵelengedwa , mukuzindikila kuti Paulo wagwila mau a “ malemba oyela , ” kapena kuti Malemba a Ciheberi mobwelezabweza . Dzina lake linali Jim Gardner . Pokhala munthu wangwilo , Yesu anapulumutsa anthu ku ucimo ndi imfa mwa kuwafela . NYIMBO : 127 , 101 M’Baibulo , mau akuti “ dzanja ” la Mulungu amatanthauza mphamvu zake . “ Ndimalemekeza Baibulo cifukwa ndi buku lakale , ndipo ndamva kuti anthu amaligula kwambili . Pamene tisinkha - sinkha pa zinthu zimene Yehova amatipatsa , timaona kuti Yesu akanapanda kupeleka moyo wake monga nsembe , sitikanakhala paubwenzi ndi Yehova . Paulo analemba kuti : “ Tatsimikiza kuti munthu mmodzi anafela anthu onse , cifukwatu onsewo anali atafa kale . Mu 1943 , M’bale Nathan H . Kukanakhala kuti anthu ambili amatsatila mfundo zimene tachulazo , sembe mavuto a anthu padziko anacepa . Kodi tingacite ciani kuti tipitilize kucita zimenezi ? 7 : 9 , 14 ) Conco , tiyeni tsopano tikambilane cifukwa cake Yehova anaona anthu amenewa kukhala zitsanzo zabwino pa nkhani yocita cilungamo . Kumene sanawavomeleze kuŵelenga poyela , ophunzilawo anatumiza makope a makalata kwa mamemba onse a chechi yawo . Pamapeto pake , zolengedwa zonse za kumwamba ndi za padziko lapansi zidzakhala zogwilizana monga banja limodzi . Patapita zaka 10 , mwana wa M’bale Julian , amene tachula kuciyambi kwa nkhani ino , anasintha khalidwe lake , ndi kubwezeletsedwa mumpingo ndipo tsopano akutumikila monga mkulu . Tingacilimbitse bwino cikumbumtima cathu mwa kuphunzila Baibo , kupemphela , ndi kugwilitsila nchito zimene timaphunzila . ( 1 Tim . ( 2 Maf . 13 : 20 , 21 ) Akristu oyambilila anali kukhulupilila nkhani za m’Malemba zimenezi , monga mmene ife timakhulupilila kuti Mau a Mulungu ndi oona . 4 : 17 . ( Aroma 10 : 17 ) Dzifunseni kuti , ‘ Kodi ndimapezeka pamisonkhano nthawi zonse ? ’ Kugwilitsila nchito nthawi ndi mphamvu zathu kuti tisamalile zinthu zina n’kofunika . Koma tingafunike kusintha zinthu zina pa umoyo wathu kuti tizitaila nthawi yathu yambili kutumikila Yehova Tingaphunzilepo kanthu tikaona “ maluwa akuchile . ” Tonse aŵili taphunzila kuti coonadi ponena za Mulungu n’cosavuta kumvetsa , ndipo ndi cuma camtengo wapatali . Mlongo wina dzina lake Elvira akumbukila bwino zimene zinacitika atasiyana maganizo na mnzake Giuliana . Elvira anati : “ Pamene iye ananiuza kuti zimene nacita zamukhumudwitsa , n’nadziimba mlandu . Inunso monga mmodzi wa atumiki a Yehova , mosakaikila mumaona kuti kugwila nchito yopanga ophunzila ndi mwai wamtengo wapatali . Ndithudi , pamene tikonzekela Cikumbutso , tingacite bwino kuganizila mmene nsembe ya Yesu inatimasulila ku ucimo ndi imfa . Sin’naloŵepo sukulu yophunzitsa cinenelo cimeneci . Zikwangwani zimenezo zinaikidwa pa malo amene mseu unadutsa pa njanji . 7 : 19 ; Zef . 1 : 18 ) Kodi inu mungamvele bwanji ngati muli pafupi kufa , ndipo mwazindikila kuti munataya cuma ceni - ceni pofuna kudziunjikila “ cuma cosalungama ” ? Kodi tingatsanzile bwanji kukoma mtima kwa Mulungu ? Timavutika kuleza mtima maka - maka ngati tiyembekezela kuti zinthu zimene timakonda zicitike . N’ciani cingatilepheletse kulandila uphungu ? José na Rose ali pamodzi ndi Tony na Wendy Tikalibe kuphunzila za Yehova , mwina tinali kucita zinthu zimene iye amadana nazo , ndipo mwina tikali kulimbana ndi zilakolako zoipa . Ngati ndimwe mlongo wosakwatiwa , ndipo mufunitsitsa kucitako utumiki wokhutilitsa umenewu , tikhulupilila mudzapindula na zimene iwo anakamba . Conco , pamene Aisiraeli anali okhulupilika , anacitila umboni dzina la Mulungu mokwanila . 4 , 5 . ( a ) Kodi Yesu wakhala akucita ciani kuyambila 1914 ? Muyenela kupewa kuuza ena zolakwa za mwamuna kapena mkazi wanu ngakhale mwanthabwala cabe , kapena kudandaulila ena za khalidwe la mnzanuyo limene mumakhumudwa nalo . M’zaka 100 zoyambilila , anthu ambili anali kukonda zosangulutsa . Iwo anali kukamba kuti : “ Tiyeni tidye ndi kumwa , pakuti mawa tifa . ” ( 1 Akor . Dzifufuzeni kuti muone mfundo zimene m’mayendela . Chris anazindikila kuti anali na vuto la kunyada ndi kusafuna kuuzidwa zocita . Anthu amacita kupanga mpikisano kuti adziŵike kuti io ndi aukali kwambili , ankhanza ndiponso aciwelewele . 2 : 3 ; Luka 9 : 48 . Ena amacita zimenezi kuti apewe cilango , kapena pofuna kudyela ena masuku pamutu . Kuti mupambane pa nkhondo yoteteza maganizo anu , mufunika kuzindikila kuopsa kwa mauthenga osoceletsa a Satana ndi kupeza njila zodzitetezela 16 : 24 , 27 ) Iwo sanazengeleze kapena kuwayawaya . Pa Pentekosite mu 33 C.E . , atumwi anayamba kutsogolela mpingo wacikhiristu . “ Pemphanibe , ndipo adzakupatsani . ” — Luka 11 : 9 . Pa tsamba 2 la magazini amene ndakubweletselani pali nkhani imene ionetsa kuti kukhulupilila Yesu kungatithandize kuti tikapeze moyo . ( Onani palagilafu 19 ) Atate anali ndi famu kudela linalake la kumidzi . Kumeneko anasiya abululu ŵake , zinthu zabwino za mumzinda wotukuka umenewo wokhala ndi mamaliketi na mashopu , komanso nyumba yake yabwino , mwina yokhala na mapaipi a madzi . Yesu anakamba kuti mzimu wa Mulungu ungatikumbutse zinthu zimene tinaphunzila . ( Yoh . N’cifukwa ciani Mulungu anaona kuti iwo anam’tumikila ndi mtima wathunthu ? Ngati palipano mnzanu wa m’cikwati safuna kukhala wotsatila Khristu , sindiye kuti muli na cifukwa comveka copatukilana kapena kusudzulana naye . Ambili masiku ano samvela cisoni akacimwa , conco samvetsetsa cifukwa cake ife anthu tifunikila dipo . Kuonjezela apo , coonadi ca m’Mau a Mulungu cimatimasula ku zikhulupililo ndi zamatsenga zogwilizana ndi imfa . — Onani bokosi yakuti “ Kodi Akufa Ali Kuti ? ” Komabe , io anayesa Yehova monga mmene iye amatipemphela kuti : “ Ndiyeseni conde . . . kuti muone ngati sindidzakutsegulilani zipata za kumwamba ndi kukukhuthulilani madalitso oti mudzasoŵa powalandilila . ” — Mal . Kuphunzila Cituvalu sikunali kopepuka . 16 : 3 ; 20 : 18 . N’cifukwa ciani zimene timaikapo maganizo ni nkhani yaikulu ? Ndipo ena amene atumizidwa kukacita upainiya amabwela kupempha malangizo . Ngati takumana ndi vuto lalikulu , tifunika kudekha kuti ticite zinthu mwanzelu . Kodi kudela lanu eninyumba angakhumudwe mutacita zimenezi ? ( Yoh . 18 : 1 - 8 ) Atafunsidwa mu Khoti Yapamwamba ya Ayuda , iye molimba mtima anavomela kuti anali Kristu ndiponso Mwana wa Mulungu , ngakhale kuti anadziŵa kuti mkulu wa ansembe anali kufunafuna cifukwa coti amuphele . Tisamaiŵale kuti Yehova amafuna kuti tizimumvela na mtima wonse na kukhala wodzipeleka kwa iye yekha . Komabe m’kupita kwa nthawi , buku lochedwa “ Let Your Name Be Sanctified , ” limene linafalitsidwa mu 1961 , linati Naboti anali kuimila odzozedwa , ndipo Yezebeli anali kuimila Machalichi Acikristu . Yehova amaseŵenzetsa mpingo ndi akulu kuti aumbe aliyense wa ife . 20 : 1 , 2 ; 28 : 10 , 11 ; 32 : 2 . Conco , anamuyamikila ndi kumukhululukila . Koma onse , kuphatikizapo ofalitsa okalamba , amayesetsa kulalikila paliponse m’gawo la mpingo wawo . Sitinayembekezele zimenezo . Iye analonjeza kuti padzakhala “ mbeu ” imene idzaononga Satana ndi kucotsa mavuto amene amabwela cifukwa ca ucimo wa Adamu . — Ŵelengani Genesis 3 : 15 . ( Deut . 33 : 5 ) Koma anthu sanakhutile ndi ulamulilo wa Yehova amene anali Mfumu yao yosaoneka . yacingelezi ya December 22 , 2000 , tsamba 9 . Colinga canu ciyenela kukhala kum’thandiza mwacikondi ndi mokoma mtima . Conco , dzifunseni kuti , ‘ Kodi izi zikanakhala kuti zacitikila ine , sembe nifuna kuti ena azicita nane zinthu motani ? ’ — Mat . MUZIGANIZILA ZINTHU ZABWINO . 26 : 18 , 19 . Amene anali otsatila a Yesu odzozedwa ndiponso amene anakhalabe ndi iye m’masautso ake , adzalamulila pamodzi naye kumwamba . ( Afil . ( Chiv . 19 : 11 - 16 ) Conco , n’zoonekelatu kuti Yesu adziŵa tsiku limene Aramagedo idzabwela . Iwo sanafunike kukhala acinyengo . Pa cocitika capadela cimeneci , Alevi anaimba nyimbo yacitamando imene mbali yake ina timaiŵelenga pa 1 Mbiri 16 : 31 , pamene pamati : “ Anene pakati pa anthu a mitundu ina kuti : ‘ Yehova wakhala mfumu ! ’ ” “ Conco tisaleke kucita zabwino , pakuti pa nyengo yake tidzakolola tikapanda kutopa . ” — Agal . Kwa Aisiraeli amene anali ku ukapolo , iye anakhala Mpulumutsi , Mtetezi , Mtsogoleli , ndi wosamalila zosoŵa zao zonse zakuthupi ndi zakuuzimu . T . Koma kumatanthauza kukhwima kuuzimu ndi kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova . Ndiyeno pang’ono ndi pang’ono ndinayamba kuwathandiza kuti popemphela azichulanso mfundo zofunika zopezeka mpemphelo lacitsanzo kuti mapemphelo ao azikhala atanthauzo . ” Kodi mau a Paulo a pa Afilipi 4 : 6 , 7 amatitonthoza bwanji ? Yankho lake lingatithandize kudziŵa mmene tingam’thandizile . — Ŵelengani Miyambo 20 : 5 . Vesi 9 Mdyelekezi , “ amene akusoceletsa dziko lonse lapansi , ” anaponyedwa padziko lapansi . Iye anapatsidwa mwai womulipilila maphunzilo ndipo makampani ambili oyang’anila zovinavina m’dziko la United States anali kum’gwilitsila nchito . Muyenelanso kupemphela kwa Yehova . M’bale wina wa ku Japan analemba kuti : “ Pamene ndinali ndi zaka 14 , ndinapita muulaliki ndi mkulu wina ndipo iye anaona kuti sindinali kusangalala ndi utumiki . Alan ndi wacinyamata , koma angakwanitse kuganizila mavuto amene sanakumanepo nao . ( 2 Akor . 2 : 11 ) Kuwonjezela apo , cifukwa ca zimene timaŵelenga m’Baibo , monga m’buku la Yobu , timadziŵa cifukwa cake Mulungu amalolela kuti tizivutika . Tonse timakhudzidwa ndi mavuto amenewa . M’Baibo timaŵelenga kuti : “ ‘ Ndiyeseni conde , . . . kuti muone ngati sindidzakutsegulilani zipata za kumwamba ndi kukukhuthulilani madalitso oti mudzasoŵa powalandilila , ’ watelo Yehova wa makamu . ” ( Mal . Mfumu Yehoasi ya Yuda analamula ansembe kuti atenge ndalama zimene anthu anapeleka kunyumba ya Yehova ndi ‘ kukonzela ming’alu ya nyumbayo paliponse pamene panali mng’alu . ’ ( 2 Maf . Onani Nsanja ya Olonda ya September 15 , 2012 , tsamba 13 - 17 pamutu wakuti “ Sukulu Zophunzitsa Atumiki a Mulungu Zimasonyeza Kuti Yehova Amatikonda . ” Khalidwe lina limene tifunika kukhala nalo pamene tikukonzekela kudzakhala m’dziko latsopano ndi mzimu wokhululuka . Komabe , m’buku latsopanoli zilembo zake zinalembedwa kucoka pamwamba kupita pansi potengela kalembedwe kofala ka m’manyuzipepala ndi mabuku ena a Cijapanizi . Akakhala mumzinda wothaŵilako , munthu wopha mnzake mwangozi anali kukhala wotetezeka . Inenso ndinacita nao zinthu zoipa . N’cifukwa ciani Mkhristu sayenela kudabwa ngati waona kapena kucitilidwa zinthu zopanda cilungamo mumpingo ? Koma Yesu pofuna kumukhazika mtima pansi , anamuuza kuti : “ Mwanawe , limba mtima . ” Iye ndiye bwenzi labwino koposa onse . Araceli : Cifukwa cakuti anali kundivutitsa kunyumba ya masisitele , ndinakhumudwa ndi cipembedzo canga . Ndiye cifukwa cake timakonda kudya zakudya zopatsa thanzi . TAYELEKEZELANI kuti muli ku mwambo wa cikwati , ndipo okwatilanawo akuyang’anana ndi kumwetulilana monyadilana . ( Ekisodo 3 : 15 ; Salimo 83 : 18 ; 148 : 13 ; Yesaya 42 : 8 ; 43 : 10 ; Yohane 17 : 6 , 26 ; Machitidwe 15 : 14 ) Pogwilitsila nchito mzimu wake , Yehova anauzila olemba Baibulo kuti alembe dzina lake nthawi masauzande ambili m’mipukutu yakale . Iye anati : “ Cuma capadela cimene anaciika m’manja mwakoci , ucisunge mothandizidwa ndi mzimu woyela umene uli mwa ife . ” ( 2 Tim . Komabe , sitiyenela kukakamiza anthu kuti adziŵelenga ndi kuphunzila Baibulo . Ndiye cifukwa cake Akhiristu acicepele sacita cinyengo kuti apeze magiledi abwino ku sukulu . M’malomwake , popeza Yesu anali wozindikila , anadziŵa kuti Natanayeli anali woona mtima . Koma Baibo imatithandizanso m’njila zina . Kodi mabwenzi a Mulungu adzalandila madalitso otani ? Komabe , iye amaonetsabe ‘ cifundo kwa osayamika ndi kwa oipa . ’ Ŵelengani Mateyu 6 : 27 . Patapita zaka ziŵili , masisitele anatitumiza kunyumba ina yaikulu ya masisitele ku Zaragoza , kumenenso anali kusungila okalamba . Mu 1473 B.C.E . , Yoswa anatuma azondi aŵili kuti akazonde Yeriko , ndipo kumeneko anapeza mkazi wina wochedwa Rahabi amene anali hule . Maggy * mlongo wa ku Australia , anafotokoza zimene zinali kucitika pamene anayamba cibwenzi ndi munthu wosakhulupilila . NKHANI YAIKULU YA M’BUKULI Kodi Mumaona Kufunika Kophunzitsa Ena ? Ambili anali kumutsutsa , ndipo ena anali kum’zunza . ( Mac . * Cifukwa cakuti bukuli linali limodzi mu mzinda wonse wa Tokmok , tinali kucita kukopela na manja kuti tikhale nalo . Kumeneko , tonse timaphunzitsidwa zinthu zofanana . Baibulo limatiuza kuti mosiyana ndi atate ao anawa anali “ kupotoza ciweluzo . ” — Ŵelengani 1 Samueli 8 : 1 - 5 . Izi zinam’khumudwitsa kwambili Sara wosabeleka ! Zimanipatsa cidalilo cakuti Yehova amatsogoleladi gulu lake , ndipo zolinga zake zidzacitika . ” Conco nthawi zonse tiyenela kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova . Komanso acikulile ambili akugwilitsila nchito nthawi yao ndi mphamvu zao potumikila Yehova . ( Mateyo macaputala 5 - 7 ) Poyamba sindinali kumvetsetsa zimene Yesu anatanthauza pamene anakamba kuti “ odala . ” ( b ) Ni zinthu ziti zimene Yosefe sanakambe kwa wopelekela cikho ? 103 : 13 ) Mwana sangayembekezele kuti kholo lake lizimucitila mwamsanga ciliconse cimene wapempha . Imeneyi ndi mfundo yolimbikitsa kwambili kwa anthu onse amene anasiya coonadi kuti abwelele kwa Yehova mwamsanga . Webusaiti ya jw.org ili ndi mfundo zolondola zokhudza zikhulupililo za Mboni za Yehova ndi zimene zimacita . Anthu ambili amene amaganiza zopita ku maiko ena amadziŵa kuti cosankha cao cingabweletse mavuto . Kodi Hana anapeza kuti thandizo pamene anali na nkhawa ? Baibulo limanena kuti Yesu ndiye “ cithunzi ceniceni ca Mulungu weniweniyo . ” ( Aheb . Iwo afunika kuphunzila za Yehova ndi kum’konda , komanso afunika kudziŵa zimene Mulungu amafuna kuti io acite . Zimene iwo analonjeza zinacititsa kuti ana awo ayambe utumiki wapadela pacihema . “ Kukhala na umoyo wosalila zambili kwanithandiza kukhala womasuka ndi kuika maganizo anga pa zinthu zofunika kwambili , ” anatelo Federico , m’bale wokwatila wa zaka za m’ma 40 , amene ni wocokela ku Spain . Dzina la Mulungu linalembedwa mu mipukutu yakale ya Baibulo Koma si onse amene ndi othandiza . Kodi citsanzo ca Timoteyo cimasonyeza bwanji kuti Yehova ndi wofunitsitsa kupatsa acinyamata maudindo ? Mabaibo ena mukhoza kuwaŵelengela pa intaneti kapena mungacite daunilodi kuti muziwaŵelengela pa kompyuta , pa tabuleti , kapena pa foni yanu . Yosefe , kalipentala wa ku Nazareti , anali atate a Yesu omulela . Mtumwi Paulo anali kudziŵa bwino kuopsa kwa mauthenga osoceletsa a Satana . Popeza Mulungu anatiloŵetsa m’gulu lake loyela limene limatisamalila na kutiteteza , tili na udindo wothandiza kuti gululi likhalebe loyela . Ndithudi , zikanakhala kuti Khristu sanaukitsidwe , sembe sakulamulila monga Mfumu yathu , ndipo ulaliki wathu wokamba za ulamulilo wa Khristu ukanakhala wopanda phindu . 11 : 1 ; 2 Ates . Monga otsatila a Kristu , tiyenela kuzindikila kuti palibe nchito ina yapamwamba imene ingapose nchito yolalikila uthenga wabwino . Nanga bwanji za cinenelo , kodi iye wapita patsogolo ? ( Yuda 14 , 15 ) Ciwawa cinali ponse - ponse . Patapita nthawi , ndinakumana ndi Angelines , amene tinali kukhala naye pafupi , ndipo anakhala mnzanga . 12 : 2 , 3 ; 1 Pet . Malangizo acindunji amenewa , kuphatikizapo tsiku la imfa yake , zinalembedwa m’Baibo . — Luka 22 : 19 ; 1 Akorinto 11 : 25 . Tingapeze yankho mwa kupendanso bwinobwino mau a Paulo . N’nafuna kusamuka n’colinga cakuti nisakhale m’tauni yathu , ndi kuti nisakhalenso na ambuya amene sanali a Mboni za Yehova . ( Mat . 5 : 24 ) Zimenezi si zovuka kweni - kweni . N’cifukwa ciani ophunzila anali kutha kumvetsetsa zimene Yesu anali kukamba ? Patsani mtumiki wanu mphamvu . ” — Salimo 86 : 16 . Zimene Mariya anali kukamba . N’cifukwa ciani Akristu ayenela kukhala ndi cidalilo cakuti Yehova adzawathandiza ? 12 : 6 - 8 ; Mat . 22 : 31 , 32 ; Mac . 13 : 22 ) Mau a Mulungu amakamba kuti Yehova amacita kulaka - laka nthawi pamene adzaukitsa akufa . Ena mwa abale ndi alongo anu akuuzimu akanakhadzulidwa ndi nyama zolusa kapena kukhomeledwa pamtengo ndi kutenthedwa ndi moto kuti akhale ngati zounikila usiku . Kodi muli ndi thanzi labwino kapena m’madwala - dwala ? Nthawi zambili Mulungu anali kuika maganizo ake mwa olembawo ndi kuwalola kusankha mau oyenelela kuti afotokoze uthenga wake . — Ŵelengani Chivumbulutso 1 : 1 ; 21 : 3 - 5 . Mosiyana ndi kale , io anali kucepetsa zinthu zogula . Ndili ndi zifukwa zambili zoyamikilila Yehova . Tsopano ndakhala ndikutumikila pa Beteli kwa zaka 10 , ndipo ndifuna kupitilizabe kuthandiza abale ndi alongo mwa kutumikila pa Beteli . ” “ Kudzakhala milili ndi njala m’malo osiyanasiyana . ” — Luka 21 : 11 . Ngati mphunzitsi amakonda wophunzila , sicikhala covuta wophunzilayo kuzindikila zimenezo , ndipo zimakhudza kwambili mmene iye angagwilitsile nchito malangizo amene wapatsidwa . 46 : 11 . Akulu ndi ofalitsa ena mumpingo anauza Marilyn kuti asapite , koma alongo ena anam’limbikitsa kuti apite . Iwo anafika pomulanda mabuku ophunzilila Baibo . Kumatithandizanso kudziŵa bwino njila za Yehova , ndipo tikadziŵa njila zake timayamba kumukonda kwambili . Anacita zimenezi kwa anthu monga Farao wa m’nthawi ya Aburahamu ndiponso Miriamu mlongosi wa Mose . Anthu ofika m’mamiliyoni apeza kuti masomphenya amenewa amalimbitsa cikhulupililo cawo , na kuwapatsa ciyembekezo ca tsogolo labwino . Poyamba , Baibulo linalembedwa pazinthu zosacedwa kuonongeka , monga pamipukutu yamapepala a gumbwa ndi zikopa . Mavuto amenewo ndi ( 1 ) kuzoloŵela umoyo watsopano , ( 2 ) kuyewa kunyumba [ acibale ] ( 3 ) kuzoloŵelana ndi abale a kumeneko . Mulimonse mmene zinalili , Paulo ayenela kuti anafotokoza kuti amalambila Mulungu wa Ayuda ndi kuti anali kulimbikitsa anthu onse kulemekeza boma . Anali kufunitsitsa kucita cabwino , koma cinthu cina cinali kumulepheletsa . Yesu ayenela kuti anali wosangalala kwambili pamene Atake ake “ anali kukonza kumwamba ” ndi ‘ kukhazikitsa maziko a dziko lapansi ’ . N’cifukwa ciani zimene Mateyu na Luka analemba zokhudza umoyo wa Yesu ali mwana zimasiyana ? Yesu anaika maganizo ake pa madalitso a mtsogolo . Mukhoza Kukhalabe Wodzicepetsa Ngakhale pa Ciyeso , Jan . Ganizilaninso citsanzo ca Zoila . ( 1 Mbiri 25 : 7 ) Masiku ano , tikumenya nkhondo yakuuzimu yolimbana ndi Satana ndi otsatila ake . Ngati tikumbukila mfundo yakuti Mkhiristu aliyense afunika “ kunyamula katundu wake , ” tidzalemekeza ufulu wa ena pa zosankha zawo . Pamene muzifuna - funa yesetsani kukhala odzicepetsa ndi olimba m’cikhulupililo . — w16.08 , mapeji 18 - 19 . Baibulo imakamba za atumiki ena a Mulungu amene anakamba kapena kucita zinthu zimene zinakhumudwitsa ena . Ndiyeno , iye anapeleka madinali aŵili kwa mwininyumba ya alendo . Kwa zaka zambili , abusa a machechi akhala akuphunzitsa kuti munthu ali na mzimu umene sukufa . 20 : 18 - 21 ) Mose anakwela m’phililo , ndipo anakhalamo kwa nthawi yaitali . Kodi kulimba mtima kunamuthandiza bwanji mlongo wina wacicepele kukwanilitsa zolinga zake ? Kenako mnzake akumumenya kumsana kuti nyamayo icoke . M’malo mosiya lamulo langwilo la Mau a Mulungu , iye amalimbikila kutsatila ziphunzitso zake . Ndi malingalilo a mtima ati amene angatilepheletse kumvetsela kwa Yehova ? Mumandinyansa ndi cipembedzo canuci . ” Iye amatiuza colinga cake , kuonetsa kuti amasamala za anthu . Ni mmenenso akulu , apainiya , na atumiki a pa Beteli amamvelela akayamikilidwa cifukwa cotumikila mokhulupilika . Nayenso Peter , amene anadzakhala mwamuna wa Mlongo Joyce , anamvela pempho yakuti “ Galamukani . ” Iye “ anayamba kuganizila zoyamba upainiya . ” Yesu anali munthu wangwilo . Tingayamikile bwanji cikondi ca Mulungu ? Cifukwa cakuti munthu amene sali pabanja amakhala ndi mipata yambili youzako ena uthenga wabwino . Nimanyadila kukhala m’gulu la anthu a Yehova , ndipo nimamuyamikila cifukwa ca mwayi umenewu . ” Koma n’zokayikitsa kuti anali kumvetsetsa zimene zinali kuŵelengedwa . Nanga Yesu anayankha bwanji funso limene Afarisi anamufunsa ? Monga Akristu oyambilila , timayamba kukhulupilila Yehova ndi kukamba molimba mtima pa cocitika ciliconse . — Machitidwe 4 : 17 - 20 ; 13 : 46 . Kodi n’zotheka kuuza Yehova m’pemphelo mavuto athu ndi kukhala ndi mtendele wa m’maganizo , tili ndi cidalilo cakuti tacita mbali yathu ndipo iye adzasamalila zotsala ? Amene amadzipeleka kukagwila nchito pa Beteli kwa tsiku limodzi kapena angapo pa mlungu , amadzipezela okha zofunika paumoyo . Kodi kukangana naye kungakonze zinthu ? Imati : “ Munthu wanzelu zopindulitsa adzaopa dzina [ la Mulungu ] . ” Ndithudi , goli la Yesu ni lofewa . ( c ) Kodi muganiza kuti Mdyelekezi amamva bwanji mtumiki wa Yehova akacita chimo lalikulu ? Tinali na colinga copitiliza kucita upainiya kwa nthawi yaitali mmene tikanathela . Tikakhala pa chuti , tinali kucita pisiweki yothyola zipatso kuti tizipezako ndalama . Poyamba iye sanakondwele kuti amai ake anapita , koma pamene amai ake anabwela kukaceza sanali wosangalala kuwaona . Mosakayikila , iwo anapindula kwambili kukhala ndi Petulo cifukwa anali munthu wodziŵa zambili ndi wodziŵa bwino Malemba . N’zoona kuti mumpingo sitingayembekezele kupeza munthu wocita zoipa ngati Maaka . Koma nthawi zina mungafunike kucita zinthu molimba mtima ngati Asa . Kodi mpingo ungalemekeze okalamba pakati pao m’njila ziti ? N’ciani cimene tikuphunzila pa citsanzo ca mtumwi Paulo pankhani yokhala oyamikila ? N’cifukwa ciani sitifunika kunyalanyaza zofooka zathu ? Yesu anali wodzipeleka kwambili panchito yake yolalikila ndi kuphunzitsa . Zimene analemba zinakhudza kwambili Martin Luther , William Tyndale , ndi John Calvin . — wp16.6 , mapeji 10 - 12 . Ndipo tsiku na tsiku zinthu zikuipila - ipila . Pamene kwatsala masiku ocepa kuti ticite Cikumbutso , tiyenela kuganizila mafunso amene tingaseŵenzetse pothandiza ophunzila Baibo ndi anthu oona mtima kucita cidwi ndi cocitika capadela cimeneci . ( Mat . 24 : 3 ) Mwacitsanzo , iye anati : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu . ” Iwo acita zimenezi mwa kukhulupilila umboni woonekelatu wakuti Yesu ali pafupi kubwela , ndipo ndi okonzeka ponena za kubwela kwake . Popeza tinali kukhala mu Colorado pafupi na malo ocitila maseŵela osheleleka pa aisi , tinaphunzila maseŵela amenewa kuti tiziseŵelela pamodzi monga banja . Mofananamo , ngakhale kuti “ palibe munthu anaonapo Mulungu ndi kale lonse , ” Yesu Mwana wa Mulungu , “ amene ali pa cifuwa ca Atate ndiye amene anafotokoza za Mulungu . ” Kumene n’nali kutumikila kunakhala kwathu . Bungwelo linatumiza mamembala ake aŵili , Petulo na Yohane , kuti akapemphelele okhulupilila atsopano a kumeneko n’colinga cakuti alandile mzimu woyela . ( Mac . N’cifukwa ciani Mulungu anatipatsa mtima wofuna kukhala ndi moyo “ mpaka kale - kale ” ? Cimene cingakuthandizeni kuti musagonje pa ciyeso ciliconse , ni kukumbukila kuti lonjezo lanu la kudzipeleka kwa Yehova n’losasinthika . Ndipo mu August 2005 , ndinapatsidwa mwai wotumikila m’Bungwe Lolamulila . Ngati mungakonde , tikulimbikitsani kuti : “ Kwezani maso anu muone m’mindamo , mwayela kale ndipo m’mofunika kukolola . ” Kodi anthu a Mulungu anaonetsa bwanji kuti anali ogwilizana m’nthawi ya Yehosafati ? Mu 1987 , tinapita ku North Carolina kukatumikila m’dela limene kunali ofalitsa ocepa , ndipo tinapeza mabwenzi ena ambili kumeneko . Ndipo m’caputala cimeneci muli vesi lina limene limatilimbikitsa kukhala anzelu . Kuti mudziŵe zambili za Ufumu wa Mulungu , onani nkhani 8 m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . ( Ŵelengani Mateyu 6 : 9 . ) Wailesi ya WBBR imene inali ku Staten Island itagulitsidwa mu 1957 , n’nakatumikilako ku Beteli ya ku Brooklyn kwakanthawi . Pamene n’nali kukula , n’nali kukonda kuseŵela na ambuya aamuna . “ Anthu Amene Mulungu Wao Ndi Yehova , ” 11 / 15 “ Pitilizani kuyenda mwa mzimu . ” — AGAL . Rudi anatumiza adilesi yanga yatsopano ku ofesi ya nthambi ku Vienna , ndipo ofesi ya nthambiyo inatumiza adilesi imeneyo kwa alongo aŵili amishonale , Ilse Unterdörfer ndi Elfriede Löhr . Tifunikanso “ kuzindikila tanthauzo ” la zimene taŵelenga . ( Mat . Mukamatelo mumakhala ngati mukuwauza kuti “ sindikusiyani ” . 25 : 6 . Koma n’zomvetsa cisoni kuti Uziya anaononga mbili yake pamene anakhala wodzikuza . Mwacionekele , pamene zimenezi zinali kucitika , Satana anali kusangalala kwambili . — Num . 145 : 16 . Iye anakamba kuti : “ N’tatumikila ku malo osoŵa caka cimodzi cabe , Doratine , mayi wacitsikana amene n’nali kuphunzila naye Baibo , anabatizika pa msonkhano wa dela . ” N’cifukwa ciani zimenezi zacitika ? ’ DZIKO : HUNGARY Ndinapatsidwa moni wotentha , wacikondi ndipo ndinaona nkhope zomwetulila . Kodi n’koyenela Mkhristu kusintha maganizo ake pambuyo popanga cosankha ? Conco , n’cinthu canzelu kutsatila malangizo a m’Baibo kuti tizilamulila mkwiyo na kupewa mtima wapacala . Mmodzi wa iwo anali Eduard Varter . Iye anabatizika mu 1924 ku Germany . ‘ Tamvelani Maloto Awa ’ YOSEFE anayang’ana kum’mawa ndi mtima wacisoni , kulakalaka kuthawa amalonda amene anali nao . Timakhululukidwa macimo “ Ndipo anthu anga ochedwa ndi dzina langa akadzicepetsa n’kupemphela , n’kufunafuna nkhope yanga , n’kusiya njila zao zoipa , ine ndidzamva ndili kumwamba n’kuwakhululukila chimo lao . ” — 2 Mbiri 7 : 14 . Ngakhale kuti papita zaka 63 , ndimakhumudwabe . ” 12 , 13 . ( a ) Monga wophunzila , ndi mtima wotani umene Elisa anali nao ? Zimene zinacitikila Ulf , zimatikumbutsa mfundo yakuti tilibe mphamvu zonse zoteteza thanzi lathu . Kodi zocita za ampatuko zinakhudza motani Akristu a m’nthawi ya Paulo ? Yesu asanabwele padziko lapansi , Yehova anagaŵila anthu nchito yokhutilitsa . Motoka na kalavani yathu Limatanthauza kuti munthu amene amagwila nchito popanda kupuma sasangalala ndi nchito yake cifukwa cakuti amatopa kwambili . Inde , Yehova amakondwela ngako na munthu wodzicepetsa . TSAMBA 17 Ngati mumakhala kudela kumene anthu amakonda zacipembedzo , mungayambe makambilano anu mwa kufunsa kuti : “ Ngati mngelo akamba ndi inu , kodi mungamvetsele zimene akukuuzani ? Koma pa zaka 13 , zinthu zinasintha kwambili . Tingacite ciani kuti tikhale ndi makhalidwe abwino ngati amene Yehova ali nao ? Motelo , “ Gogi ” wochulidwa mu ulosi wa Ezekieli kapena m’buku la Chivumbulutso , si Satana . ( Yobu 7 : 16 ) Mwinanso mumamvela mofanana ndi mmene Luis , mwamuna wa zaka za m’ma 80 , amamvelela . Iye anakamba kuti : “ Nthawi zina nimaganiza kuti cimene catsala ni kufa cabe . ” Ufumu wa Mulungu ukulalikidwa padziko lonse m’zinenelo zambili GWILITSILANI NCHITO MFUNDO ZA M’BAIBO KUTI MUPANGE ZOSANKHA ZANZELU ( 1 Akor . 13 : 4 ) Kukamba zoona , pamafunika kuleza mtima , kukoma mtima , ndi kudzicepetsa kuti tipitilize kulalikila uthenga wa Ufumu . • Moyo wopanda mavuto ndi zoipa udzakhalako ? Masiku ano , anthu mamiliyoni ambilimbili amavutika ndi njala cifukwa ca ulamulilo woipa wa anthu . ( Ŵelengani Mateyu 23 : 8 , 9 . ) 15 : 13 ; 17 : 22 . Sitifunika kucita kuphwanya malamulo a Mulungu kuti tidziŵe kuopsa kocita zimenezo . Tiyelekeze kuti a Inoki ndi a Mboni , ndipo akumana ndi a Yohane . 27 : 11 ) Kupilila mavuto kumatithandiza kukhala “ ovomelezeka ” komanso kumatipatsa ciyembekezo . Ena mwa anthu amene tinali kukhala nao pafupi , anaona kuti nayamba kusintha . Iwo anati : “ Araceli , pitiliza kucita zimene ukucita . ” Nanga bwanji ngati woyang’anila dela kapena mkazi wake , ndi wodwala ku cipatala ndipo mwina afunikila opaleshoni ? Aisiraeli analandila zinthu zabwino zambili kucokela kwa Yehova . Usadzapeleke ana ako aakazi kwa ana ao aamuna ndipo usadzatenge ana ao aakazi ndi kuwapeleka kwa ana ako aamuna . Conco , n’nafunikanso kupita kukatumikila ku zisumbu zina kwa zaka zingapo . Anatilangizanso kuti tikatsiliza kuphunzila buku la Zimene Baibulo Ingatiphunzitse na wophunzila amene akupita patsogolo , tiziyamba naye buku lakuti “ Khalanibe M’cikondi ca Mulungu , ” ngakhale kuti munthuyo ni wobatizika . Kudzipeleka ndi pemphelo lolonjeza Yehova kuti mudzam’tumikila kwamuyaya . Kuti tipeze yankho , tiyeni tikambilane zimene zinacitika zaka zambili m’mbuyomo . M’malomwake , tidzayesetsa kutsatila mwamsanga malangizo aliwonse atsopano amene Yehova amapeleka kupitila m’gulu lake . N’ciani cionetsa kuti Baibo ni buku ya dongodolo ? Iye anafotokoza kuti : “ Ndinali kukamba ndi Yehova tsiku lililonse ngakhale ndikafuna kupanga zosankha zing’onozing’ono . Kucokela nthawi imeneyo , iye analeka kubisala akaona Mboni za Yehova . Caka cimodzimodzi cimene m’bale Skinner anafika ku India , ndi pamene nchito yolalikila inali itangoyamba muno mu Zambia . idzabweletsa bwanji madalitso mu ulamulilo wa Ufumu wa Mulungu ? CIKUTO : Alongo aŵili agwilitsila nchito buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , polalikila kwa azimai aŵili acindebele amene avala zovala zacindebele . Ambili amangowanyalanyaza , koma iwo sacokapo , ndipo amaonetsa nkhope zacimwemwe kwa aliyense amene wawayang’ana . 8 - 10 ) Umu ni mmene Yehova amacitila zinthu . Makhalidwe amenewa ali monga mizati yolimba imene imagwila nyumba . M’malomwake , amakumbuka Yesu panthawi ya Krisimasi ndi Isitala basi . Yohane analemba kuti : “ Anthu onse amucitila umboni Demetiriyo . . . ▪ Zimene Tiphunzilapo pa Fanizo la Matalente Kwa ine , zinalidi zovuta kumvetsa . Ndinali kugona m’makwalala , m’mapaki , kapenanso kwa anzanga . Ngakhale kuti atsogoleli a cipembedzo anayesa kutentha Mabaibulo onse amene anapeza , Baibulo limene Tyndale anamasulila linafalitsidwa kwa anthu ambili . Mabaibo ena ali na zinthu zimene zingakuthandizeni kuyelekezela mavesi amene muŵelenga ndi mavesi ena a m’Baibo , kapena kuyelekezela mmene Mabaibo ena anamasulila mavesiwo . Ena amaona kuti Mulungu amakonda anthu onse mosasamala kanthu za zimene io amacita . Davide anali na zonse zimenezi . Koma anakhalabe na mtima wodzicepetsa mu umoyo wake wonse . Popeza timagwilizana ndi gulu la Mulungu , ndife osangalala kugwila nchito yopatulika yolengeza uthenga wabwino wa Mulungu . Mungacite izi pamene muli mu ulaliki kapena pamene muli ku sukulu . ( Aroma 5 : 19 ) Ucimo ndi imfa zimene tinalandila kwa Adamu zinakhala adani oopsa amene anthu opanda ungwilo sangazipewe . Iye analola Adamu , Hava ndi Satana kuonetsa mmene anali kuonela Mulungu . Ku misonkhano imeneyi timatsitsimulidwa mwauzimu ndi kulandila malangizo kudzela mu gulu lake . Popeza tsopano ndasintha khalidwe langa , mwana wanga nayenso wasintha . Kodi Sara adzacita ciani ? Okopa Baibo aciyuda analakwitsa zinthu zing’ono - zing’ono poikopa . Inoki ayenela kuti analimbikitsidwa kwambili ataphunzila za Abele , amene anaphedwa cifukwa colambila Yehova m’njila yoyenela . Ŵelengani Miyambo 22 : 4 . Koma tikaganizila mmene zinthu zinalili , timaona kuti Yehova anali nafe . Cifukwa cogwilitsila nchito zimene amaphunzila , ofalitsa oposa 7 miliyoni ndi okonzeka kulalikila ndi kuphunzitsa m’njila imene imafika pamtima “ anthu osiyana - siyana . ” — Ŵelengani 1 Akorinto 9 : 20 - 23 . Ngakhale kuti Yosefe sanaiwale mavuto amene anakumana nawo , sanakhumudwe . ( Mateyu 22 : 35 - 39 ) Komabe , Baibulo imakamba kuti anthu onse amabadwa opanda ungwilo cifukwa ca ucimo wa Adamu . Atatsiliza maphunzilo , iwo anatumizidwa kuti akapitilize kutumikila ku Madagascar , ndipo anakondwela maningi . Katswili wina wa Baibo analemba kuti ngati wakupha munthu sanaonane na akulu , “ anali kuika moyo wake paciwopsezo . ” ( 1 Maf . 3 : 9 ) Caciŵili , pendani Mau a Mulungu na kufufuza malangizo m’zofalitsa za kapolo wokhulupilika kuti mukwanitse kusiyanitsa pakati pa “ cisoni ca dziko , ” na “ cisoni cogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu , ” kapena kuti kulapa kweni - kweni . ( 2 Akor . Pambuyo podzifufuza mwa kugwilitsila nchito mafunso awa , musakhumudwe ngati mwaona kuti cikhulupililo canu cayamba kufooka . Inde , mayeselo amene timakumana nawo ndi amenenso anthu ena amakumana nawo . ( b ) N’ciani cinathandiza otsatila a Yesu kumvetsa coonadi cofunika ? Tikalimbitsa cikhulupililo cathu tsopano , tidzaona Yehova kukhala Munthu weniweni amene ndi wofunitsitsa kutithandiza . ANAKHULUPILILA MALONJEZO A MULUNGU M’zaka zaposacedwa , m’maiko ambili mwakhala mukubwela anthu oculuka othaŵa kwawo . Kodi thandizo lalikulu limene Yehova amatipatsa ni liti ? M’zaka za kumbuyoku , tinali kukhulupilila kuti Yehova anali wokhumudwa ndi anthu ake cifukwa , pa nthawi ya nkhondo ya dziko lonse , anali atabwelela m’mbuyo pa nchito yolalikila . N’cifukwa ciani tiyenela kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova nthawi zonse ? N’zoona kuti mapemphelo a anthu ena a m’Baibulo anayankhidwa mozizwitsa . Patsiku latsoka Yehova adzamupulumutsa . Mau akuti “ mwana wa , ” angatanthauze “ mpongozi wa . ” ( Gen . 17 : 24 - 27 ) Mdulidwe unali cizindikilo cimene cinali kusiyanitsa mbadwa za Abulahamu , anthu okha amene anali paubale wapadela ndi Yehova . Sanaphenso nkhosa zawo zonenepa bwino . Pambuyo pa msonkhano wacigawo , banja lina linalemba kuti : “ Msonkhanowu watikhudza mtima kwambili . Ndikumbukila bwinobwino mfundo zolimbikitsa zimene abale amenewa oimila likulu la Mboni za Yehova ananena . “ Mpando wacifumu unaoneka uli pamalo ake kumwamba , wina atakhalapo . ( 1 Akor . 10 : 12 ) Conco , n’kofunika kwambili kuti nthawi zonse tizisanthula mtima wathu , kukaniza maganizo oipa , na kupewa mzimu wonyada . — Agal . 5 : 26 ; ŵelengani Akolose 3 : 5 . 21 : 25 ) Ngakhale kuti otsatila a Yesu a m’nthawi ya atumwi anali kudziŵa zambili za Yesu , munthu wangwilo kuposa zimene ife tidziŵa , sitili osoŵa kuuzimu . Sacita zinthu mopitilila malile , amaganiza bwino , ndi wadongosolo , ndipo ndi wololela . Madzi oundana akasungunuka , zingapangitse nyanja zing’onozing’ono kudzaza ndi kusefukila cakuti anthu mamiliyoni ambili angakumane ndi mavuto aakulu . Mwacitsanzo , pamene Natanayeli anadziŵa kuti Yesu anakulila ku Nazareti , anakamba kuti : “ Kodi mu Nazareti mungatuluke kanthu kabwino ? ” Mwacikondi tikukupemphani kuti muwafikile kudela lanulo kapena lembelani ofalitsa magazini ino . [ Cithunzi papeji 7 ] Munthuyo anali mneneli wokhulupilika Samueli , amene Yehova anamutuma kukadzoza mmodzi wa ana a Jese kuti akhale mfumu yotsatila ya Isiraeli . Cifukwa ca zimenezi , kacisiyo anali wokongola kwambili pamaso pa Yehova , ndipo anali kukongoletsa malo oikapo mapazi ake . Kukamba mau oyamikila kungakuthandizeni kupeza anzanu abwino . M’bale amene akukalamila udindo amakhala wopanda cifukwa comunenezela mwa kupewa kusaona mtima ndi cidetso . [ Mau apansi ] Onani nkhani yakuti , “ Akristu Amalambira Mumzimu ndi M’choonadi ” ndi yakuti “ Amayendabe M’choonadi ” mu Nsanja ya Olonda ya July 15 , 2002 . Pezani nthawi yabwino ndi malo oyenelela kuti muwalangize , ndipo citani zimenezo mokoma mtima . Kukamba zoona , anthu oona mtimawa anafunikila cakudya ca kuuzimu m’cinenelo cao . 12 TENGELANI CIKHULUPILILO CAWO | SARA Kodi nimaipidwa ndi acibululu a mwamuna kapena a mkazi wanga , olo kuti iye amawakonda kwambili ? Anasankha Rute kukhala mu mzele wa makolo a Mfumu Davide ndiponso Mesiya . — Rute 4 : 13 - 17 ; Mateyu 1 : 5 , 16 . ▪ Lolani Yehova Kulimbitsa ndi Kuteteza Cikwati Canu Anthu ambili ali yakali - yakali kufuna - funa zinthu zakuthupi cakuti ‘ sazindikila zosoŵa zawo zakuuzimu . ’ ( Mat . ( Miyambo 1 : 8 ) Pa kulambila kwanu kwa pabanja , mungathandize ana anu kupitiliza kuphunzila za Yehova ndi Baibulo . * Cifukwa ca zimenezi , amalephela kulamulila thupi lake . Mnyamatayo atafika pamphambano ya msewuwo , mkaziyo anamuyandikila , ndipo anali atavala zovala za uhule . N’ciani cinawathandiza kukhalabe okhulupilika kwa Yehova ? 26 : 15 ; 54 : 2 . Kodi tingaseŵenzetse bwanji malangizo a pa Afilipi 2 : 1 - 4 ? Cisautso cacikulu cikadzayamba , odzozedwa a m’gulu la anamwali opusa adzadabwa kwambili akadzaona kuonongedwa kwa Babulo Wamkulu . Mwina mungamve monga mmene mtumwi Paulo anamvelela . Mmene zinthu zilili paumoyo wanu zingakhudze zimene mumapeleke kwa Yehova . N’zolimbikitsa kudziŵa kuti “ lonjezo loloŵa mu mpumulo [ wa Mulungu ] lidakalipo . ” Kodi mungakonde kuiŵelenga ? Khalani maso , khalani chelu , pakuti simukudziŵa pamene nthawi yoikidwilatu idzafika . ” Niyembekezela mwacidwi kudzawaonanso ali na thanzi labwino akadzaukitsidwa . — Mac . 24 : 15 . Mukadzipeleka kwa Mulungu , ndiye kuti mwalonjeza kuti mudzacita cifunilo cake kwamuyaya . Paulo analangiza Akhristu kuti azikamba mau “ olimbikitsa monga mmene kungafunikile , kuti asangalatse owamva . ” ( Aef . Ena akumana ndi mayeso osiyanako . N’cifukwa ciani kucilikiza ulamulilo wa Yehova ni nkhani yaikulu yokhudza anthu onse ? 14 , 15 . ( a ) N’cifukwa ciani Yehova amaphunzitsa acinyamata ndi acikulile masiku ano ? N’zimene acicepele ambili sacita . N’ciani cimene Yesu anacita pamene munthu wina anam’pempha kuti amuthandize pa vuto lake ? Nsalu zimene zinali zofala kwambili zinali zaubweya . Ndipo nthawi zambili , Baibulo limakambapo za nkhosa , kumeta ubweya , ndiponso zovala za ubweya . M’delali munalibe mipingo yambili , koma munali tumagulu twambili twa ofalitsa tumene tunali patali - patali . Kodi mmene nimaonela misonkhano na zimene nimacita nikakhala pa misonkhanopo zimaonetsa kuti ndinedi munthu wauzimu ? Kodi “ kuika maganizo pa zinthu za mzimu ” kumabweletsa bwanji mtendele ? 5 : 42 . Koma zimene zinali kucitika zinandikhumudwitsa . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Pitilizani kulolelana ndi kukhululukilana ndi mtima wonse , ngati wina ali ndi cifukwa codandaulila za mnzake . ” — Akolose 3 : 13 . Nchito imeneyi inam’patsa nthawi yambili yakuti atsilize kumasulila Baibo . Anthu amene timawalalikila komanso amene timakumana nawo , amaona khalidwe lathu . Komabe , onse amene analemba Baibulo anatsogoleledwa ndi mzimu woyela . Anali kuwapatsanso zonse zofunikila paumoyo wao . Kukhala na ufulu wosankha kumathandiza anthu kusankha zocita mwanzelu tsiku lililonse . Conco , ofesi ya nthambi imawapatsa alawansi yocepa mwezi ndi mwezi , kuwathandiza kuti apitilize utumiki . Limatithandiza kukhala ‘ okonzeka mokwanila kucita nchito iliyonse yabwino . ’ 19 “ Nchitoyi Ndi Yaikulu ” Ndinazindikila kuti palibe cinthu cina m’dongosolo lino la zinthu cimene cingapose kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova . Zingakhale bwino nthawi zina kuitanako abale kapena alongo osakwatila kuti mukhale nao pa kulambila kwa pabanja . Kukumbukila mfundo imeneyi kumatithandiza “ kupilila zinthu zonse ndi kukhala oleza mtima ndiponso acimwemwe . ” — Akol . Mwacitsanzo , utali wa zaka za ukopolo unali wosiyana . Conco panthawi ina , Afarisi ena anafunsa Yesu funso ili : “ Kodi n’kololeka kuti mwamuna asiye mkazi wake pa cifukwa ciliconse ? ” — Mateyu 19 : 3 . Tinali ndi zocita zambili mu utumiki wathu m’madela amenewa . Mwina Iye angaone kuti ndinu amene muli ndi vuto . Pa zaka zonsezi , naphunzila zambili pogwila nchito pamodzi na abale a maudindo akulu - akulu . Nora nayenso wakhala akugwila nchito zosiyana - siyana pa Beteli . 8 : 30 , 31 ) Kuyamikila zimene Mulungu ndi Mwana wake anaticitila kuyenela kutilimbikitsa kupezeka pa mwambo wokumbukila imfa ya Yesu . Tikatelo , ndiye kuti tikumvela lamulo lakuti : “ Muzicita zimenezi pondikumbukila . ” — 1 Akor . Kodi Akristu ayenela kupemphela kwa Yesu Kristu ? Iye anaphunzilako kukamba citundu cawo , ndipo anayamba kuganizila za anthu ambili a mtundu wa Antandiroyi amene anali asanamveleko uthenga wa Ufumu . ( Aef . 6 : 18 ) Ganizilani za udindo wawo wopeleka cakudya cauzimu , kuyang’anila nchito yolalikila padziko lonse , ndi kusamalila zopeleka . Lonjezo la kudzipeleka kwathu kwa Mulungu n’losasinthika . Tikalonjeza , talonjeza . Cina , akazi anayamba kukhumba amuna awo , pamene amuna nawonso anayamba kupondeleza akazi awo . Mlongo Elena , amene watumikila monga mpainiya kwa zaka zoposa 25 , anati : “ Nimaona kuti nchito yolalikila ni yovuta . Adamu ndiye “ munthu mmodzi ” amene kupitila mwa iye , ucimo na imfa ‘ zinaloŵa m’dziko . ’ N’cifukwa ciani makolo afunika kupitiliza kuphunzitsa ndi kuthandiza ana awo ? Ndiye ganizani cabe mmene cimaŵaŵila ngati woticita zimenezo ni Mkhiristu mnzathu ! ( Mateyu 26 : 52 ; 2 Akorinto 10 : 4 ) Lelolino , tikumenya nkhondo imeneyi mwa kumvela Mulungu . Koma anadziŵa kuti anthu anali kucidziŵa bwino cizoloŵezi cake copemphela . ( Rute 1 : 16 ) Anthu a mitundu ina amenewa anatembenuka , ndipo mwamuna aliyense anadulidwa . Mosiyana ndi dzikoli , gulu la Yehova limafalitsa ndi kuulutsa zinthu zimene zimatithandiza kukhala ndi makhalidwe abwino . Makhalidwe amenewa adzaticititsa kukapeza moyo wosatha . N’ciani cinam’thandiza ? Ndipo Farao anawalandila ndi manja aŵili , cifukwa anali kum’dziŵa bwino Yosefe ndi kum’konda . ( Gen . Nyimbo ya Solomo imachedwa “ nyimbo yokoma kwambili . ” Koma anangokhala cete osacitapo kanthu . NYIMBO : 18 , 61 ( Aef . 4 : 32 ) Makhalidwe amenewa a umunthu watsopano adzatithandiza kutengela citsanzo ca Mulungu ndi kutonthoza anthu amene akumana ndi mavuto . — 2 Akor . USIKU wa pa Nisani 14 , mu 33 C.E . , mwezi wathunthu unaonekela ku Yerusalemu . 27 Kugwila Nchito ndi Mulungu — Kumabweletsa Cimwemwe Kuti ndikhutilitse njala yanga yakuuzimu , ndinayamba kupita ku machalichi osiyanasiyana . Atumiki a Yehova ambili anaona dzanja lake likuwathandiza kusiya zizoloŵezi zoipa monga kukoka fodya , kumwa mankhwala osokoneza bongo , ndi kuonelelela zamalisece . 6 , 7 . ( a ) Ndi nkhondo zotani zimene zacitika pa zaka 100 zapitazo ? Iye anati : “ Pamene tinali ofooka , Kristu anafela anthu osapembedza Mulungu pa nthawi yoikidwilatu . Pokhala wakupha woikidwa ndi Yehova , Yaeli anayenda mwakacetecete kufika pamene panali mutu wa Sisera . Popeza kuti amuna aŵiliwa anali olemekezeka kwambili , n’zokayikitsa kuti ananyamulako mtembowo . Mdyelekezi amacititsa kuti anthu agone mwauzimu . Ici cinasiyanitsa Adamu ndi nyama . Izo zimangocita zinthu mwacibadwa . “ Inu Yehova , conde kumbukilani kuti ndinayenda pamaso panu mokhulupilika ndiponso ndi mtima wathunthu . ” — 2 MAF . Civundikiloco kapena kuti civininkhilo citacotsedwa pa ciwiyaco , Zekariya ‘ anaonamo mkazi atakhala pansi . ’ Matenda : N’zoona kuti matenda ena , anthu akwanitsa kuwapezela mankhwala . Popeza sindinali kugulitsa zinthu zakuba , sanapeze cifukwa condiikila m’ndende . 15 : 11 ) Mfundo imeneyi ionetsa kuti n’zotheka kukulitsa cimwemwe cathu . ( August 1 , 2012 ) ; “ Kodi Mulungu Amalanga Anthu Kumoto ? ” Mlungu uliwonse , M’bale Russell anali kutumiza nkhani za m’Baibulo ku bungwe lofalitsa nkhani . Pofotokoza za munthu amene poyamba anali m’cipembedzo conyenga , Zekariya analemba kuti : “ Mneneli aliyense azidzanena kuti , ‘ Ine si mneneli . ( Luka 23 : 43 ) Ngati Yesu sanaukitsidwe , zonsezi sizikanatheka . Ngakhale kuti sitinali kudziŵa zambili zokhudza Cikristu , ine ndi mkulu wanga tinafuna kuŵaonetsa mwaulemu kuti anali olakwa . Ngati timagula zinthu zosafunikila , tikhoza kusokoneza umoyo wathu , ndipo tingayambe kukhala ndi nkhawa kwambili . Sipadzafunikilanso munthu wina kukhala mkhalapakati wathu pakati pa ife ndi Yehova . 2 : 10 - 15 ; Aroma 12 : 1 , 2 . Pamene azondi aŵili aciisiraeli anapita kunyumba kwake , iye anawauza kuti : “ Ndikudziŵa kuti Yehova akupatsani ndithu dziko lino . ” Ifenso timakumana ndi zinthu zina mu umoyo wathu zimene zimafuna kuti ticite zinthu molimba mtima . Coyamba , Ezekieli anaona mafupa “ ouma kwambili ” a anthu akufa . 3 : 21 . Coyamba , cikondi ca Kristu ciyenela kutilimbikitsa kulemekeza Yesu pa umoyo wathu . Yosefe sanafune kuti zimenezi zicitikile mtembo wa Yesu . Olo kuti titangwanike na zinthu zauzimu kapena nchito yakuthupi , tifunika kupeza nthawi yocita phunzilo laumwini ndi kulambila kwa pabanja . ( Aef . 12 : 4 ; Mat . 24 : 21 ) Paliponse m’dzikoli timaona nkhondo , makhalidwe oipa ndi kusamvela malamulo , njala , matenda , ndi zivomezi . Kuwonjezela apo , m’machalichi ambili muli msokonezo . Mwacitsanzo , kuonjezela pa ansembe ambili ndi Alevi aciisiraeli , panalinso “ akazi otumikila , amene anali kutumikila mwadongosolo pacipata ca cihema cokumanako . ” ( Eks . Koposa zonse , ngati ndise odzicepetsa , Mulungu amakondwela cifukwa iye “ amatsutsa odzikweza , koma odzicepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu . ” — 1 Pet . M’bale na mkazi wake akulalikila uthenga wabwino wa m’Baibo kwa mzimayi amene wacoka ku sukulu kumene anakatenga mwana wake . Kukhala wozindikila kumatithandiza kukhala wodziletsa ndi ‘ kusafulumila kukwiya . ’ Ndipo mu mzinda umenewu , Ophunzila Baibulo anacita msonkhano wao waukulu woyamba pa January 2 , 1927 . Kodi Akhristu ena amacita zotani zimene zapangitsa kuti asamasiyane kweni - kweni ndi anthu a ku dziko ? N’zoona kuti Yosefe anacotsedwa nchito ndipo anaikidwa m’ndende popanda cifukwa , koma Yehova anam’dalitsa . N’ciani cinathandiza Yefita kukhala wolimba pamene anali kukumana ndi mavuto ambili ? ( a ) Ndi ciyembekezo cotani cimene Akristu odzozedwa amaika m’maganizo ? Koma usadye zipatso za mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa . Cifukwa tsiku limene udzadya , udzafa ndithu . ’ ” — Gen . 12 : 4 , 5 ) Patapita zaka zoposa 200 , Mfumu Yosiya nayenso anagwilitsila nchito zopeleka za pa kacisi pokonza zinthu zina zoonongeka . — Ŵelengani 2 Mbiri 34 : 9 - 11 . 2 : 6 - 8 . Koma mwanzelu , anaganizila zotulukapo za zimene angasankhe kucita . Zimenezi ziphatikizapo “ maphwando aphokoso ndi kumwa mwaucidakwa . . . ciwelewele ndi khalidwe lotailila . ” Ndipo ngakhale kuti siticita zinthu zofanana potumikila Mulungu , tonsefe tikhoza kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu . 15 : 22 ) Janet anaona kuti afunika kugwilitsila nchito uphungu umenewu . ( Yobu 1 : 3 ) Anali wolemela , wochuka , ndipo anthu ambili anali kum’patsa ulemu . Mu January 2001 , ndiye pamene ananitumila foni imene nakamba kuciyambi kwa nkhani ino . ( Yak . 1 : 27 ) Timafunikanso kulimbikitsa ndi kutonthoza abale na alongo acikulile ndi acicepele omwe , amene ali na zothetsa nzelu , opsinjika maganizo , kapena amene akumana ndi mavuto ena . ( Miy . Ataona zimenezi , Inoki anazindikila kuti Yehova amam’konda ndi kukondwela naye . Ni mfundo yanji maka - maka imene mtumwi Paulo anali kukamba pa lembali ? Posacedwapa , amuna ndi akazi oopa Mulungu adzasandutsa dziko lapansi kukhala paladaiso . Ndipo adzathandiza anthu mamiliyoni amene adzaukitsidwa kuphunzila za cifunilo ca Yehova . KODI MUNGAKAMBE KUTI AMAYANKHA MAPEMPHELO . . . 6 / 1 Iwo amadziŵa kuti kukhala ndi makhalidwe amene Mulungu ali nawo n’kofunika kwambili kuposa cuma kapena phindu lililonse limene angapeze . Nthawi ina , Yesu anati : “ Atate , ndikukuyamikani kuti mwandimva . Ndipo zocitika za padziko lonse zimenezo zidzakhala zosiyanasiyana . Anaukitsa Lazaro tsiku lomwelo . Kodi malamulo ndiponso zigamulo za ku makhoti zatithandiza bwanji pa nchito yolalikila ? 15 , 16 . ( a ) Kodi pali msinkhu woikika umene munthu afunika kufikapo kuti abatizike ? Mofananamo , na imwe mufunika kupanga cosankha masiku ano . Ndipo zimene mudzasankha zidzakhudza tsogolo lanu . M’malo mwa njala , padzakhala cakudya cambili . Wophunzila Baibulo wina anakamba kuti kuonjezela pa “ Seŵelo ” limeneli , tumabuku tumenetu tuoneka kuti “ tunali kutsegula maso kwambili . ” Potsilizila pake mzindawu unaonongedwa ndi kukhala bwinja kwa zaka 70 . — Ezekieli 22 : 2 ; Yeremiya 25 : 11 . ( 2 Tim . 3 : 1 , 5 ) Conco , kodi tiyenela kuyamba kukaikila kukhulupilika kwa Akristu anzathu ? Iyo ikumenya nkhondo ya cilungamo ndi zolinga zabwino . ( Luka 22 : 19 , 20 ) Amene adzapezekapo adzaphunzila zambili zokhudza colinga ca Mulungu . Nchito yake inali yovuta kwambili , koma sinamucititse mantha . Kodi abale obatizika angaonetse bwanji kulimba mtima ? N’ciani cingapangitse kuti tiyambe kuwaona mosayenela abale athu mumpingo ? Auzeni ciliconse cimene mukuona ndi kumva , [ ndipo ] muzikhala wokonzeka kupitiliza kufotokoza ciliconse cimene mukuona . Apa m’pamene cikumbumtima cathu cophunzitsidwa Baibo cimathandiza . Koma n’lothandiza ngako kwa Akhristu masiku ano . Koma anthuwo anafunika kucita cina cake kuti akhalebe ndi moyo . Kale , atumiki a Mulungu ambili anali olimba mtima , ndipo anapanga zosankha zanzelu zimene zinawathandiza kuti asatenge mbali m’zandale . Tifunika kuvala zovala zimene zingalemekeze Mulungu wathu woyela , komanso abale na alongo athu . Mogwilizana ndi Mika 4 : 3 , anthu a Mulungu ‘ asula malupanga awo kuti akhale makasu a pulawo , ndi mikondo yawo kuti ikhale zida zosadzila mitengo . ’ ( Yesaya 65 : 21 - 23 ) Nanga n’ciani cinacititsa kuti asinthe ndi kuyamba kuganiza zokakhala kumwamba ? “ M’malo ambili kumene kale kunali kupezeka nsomba , sizikupezekanso , kwina zinaonongedwa kapena zikucepa kapenanso m’pamene zikuyambanso kubelekana . ” — BBC , September 2012 . Kacilembo Kocepetsetsa Kaciheberi , Na . Pa misonkhano : Anthu onse amene amabwela ku misonkhano yathu , timawalandila monga alendo anzathu amene abwela kudzadya nase cakudya cauzimu . Conco , n’naleka kukamba mau onyoza ndipo n’nayamba kulamulila mkwiyo wanga . George ndi mkazi wake Adria , ali ndi zaka pafupi - fupi 40 , ndipo anacokela ku Canada . Nthawi zonse iwo anali kukumbukila kuti Yehova amadalitsa anthu amene amapanga zosankha zabwino osati amene amakhala cabe ndi zolinga zabwino koma osacitapo kanthu . ( b ) Pankhani yopanga malonjezo kwa Mulungu , kodi tiphunzilapo ciani pa lemba la Deuteronomo 23 : 21 , 23 ndi la Masalimo 15 : 4 ? Kenako , ndinaganizila ubwino woyandikila Yehova . Ndiyeno , Abulahamu anafunika kuyembekezela kwa zaka 25 kuti mwana wake Isaki abadwe mu 1918 B.C.E . N’ciani cingatithandize kufotokoza za mumtima mwathu kwa Atate wathu wakumwamba ngati zimativuta kutelo ? Brian ndi mkazi wake Michelle , a zaka za m’ma 30 , anacoka kwao ku United States ndi kusamukila ku Taiwan pafupifupi zaka 8 zapitazo . Komabe , Yesu anakamba kuti Yehova amadalitsa anthu amene amadzipeleka cifukwa ca Ufumu . Panthawi ngati imeneyi , Baibulo limatilimbikitsa ‘ kupemphela mosalekeza , ’ komanso kuti ‘ zopempha zathu zidziŵike kwa Mulungu . ’ Ndiyeno , Yehova anaukitsa Mwana wake kukhala colengedwa cauzimu . Kuponya covalaco pamapewa a Elisa kunali ndi tanthauzo lapadela . 3 : 5 - 9 . Nanga n’cifukwa ciani timafa ? Ngakhale kuti anthu a Mulungu adzaukilidwa mtsogolo , n’cifukwa ciani sitifunika kucita mantha ? Dzina lakuti “ Yehova ” limapezeka m’mavesi oŵelengeka , ndipo m’mavesi ena a Malemba Aciheberi muli dzina lakuti “ AMBUYE , ” lolembedwa m’zilembo zazikulu . Sinidzaiŵala mmene anali kukhalila nane pamisonkhano . Tifunika kukhala na cizoloŵezi cabwino cocita phunzilo laumwini , ndipo tizifufuza mokwanila mfundo za m’Mau a Mulungu ndi m’zofalitsa zathu . Takamba zimenezi cifukwa timalalikila uthenga woyenela , umene ndi uthenga wabwino wa Ufumu . M’BUKU la Levitiko , ciyelo cimachulidwa nthawi zambili kuposa m’buku lina lililonse la m’Baibulo . M’maiko amene anthu amadzicha kuti ndi Akristu muli machalichi ndi tuakacisi twambili topelekedwa kwa Yesu , Mariya , ndi kwa anthu oyela mtima . Tsopano tiyeni tione mfundo za m’Baibulo zimene zingakuthandizeni . Caciŵili , tiyenela kucitila munthu wina zimene tingafune kuti iye aticitile . — 1 Akor . Atumiki omanga Nyumba za Ufumu amaphunzitsidwa kumanga Nyumba za Ufumu ndi kuthandiza pa zimango zosiyanasiyana m’dziko lao . Kodi tidzakhala okonzeka kucita ciliconse cotheka kuti tidzasonyeze kukhulupilika kwathu kwa Yehova ? Paladaiso ameneyu ndi mkhalidwe wauzimu wapadela umene umacititsa Akristu kukhala pamtendele ndi Mulungu ndiponso Akristu anzao . 33 : 5 . Kuti tikondweletse Yehova , tiyenela kupewa ciliconse cimene amadana naco . Komabe , pamene tili paulendowu , tiyenela kupewa zoceukitsa kapena zimene zingatisoceletse . ( 1 Yoh . 16 : 5 ) Ndipo zimenezo zinacitikadi . Ndithudi , Yehova anasiyanitsa alambili oona ndi onama pamene ‘ moto wocokela kwa Yehova , unapseleza [ Kora ndi ] amuna 250 amene anali kupeleka nsembe zofukiza aja . ’ ( Num . Yesu anali kudziŵa kuti ngakhale munthu wofunitsitsa kukhala maso angagone thupi likafooka . Ngati mwayankha kuti inde , mungacite bwino kudzipeleka ndi kubatizidwa . 13 : 35 . Ndipo thandizo yocepa imene tinalandila inatitsitsimula . Tikhoza kulimbana ndi mavuto ndi zinthu zina zoopsa mothandizidwa ndi Yehova , mzimu wake ndiponso mpingo wacikristu . NYIMBO : 69 , 57 Anthu odalilika amadalilidwa na makolo awo , anzawo , komanso mabwana awo ku nchito . Iye anaimba kuti : “ Wodala ndi munthu amene wakhululukidwa zolakwa zake , amene macimo ake aphimbidwa . • Kodi ena amavutika cifukwa ca zocita zao pamoyo wao wakale , kapena kuti Karma ? Ndipo ngakhale kuti sindinali kuwadziŵa , ndinapita kukawaona . ( 2 Mbiri 6 : 29 ) Pamene tikambitsilana ndi munthu , tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Ngati ine ndinali munthu winayo , kodi ndingafune kuti andicitile zinthu zotani ? Ndipo cifukwa ca zimenezi adani athu amayamba kutikonda . Cifukwa cokonda adani athu , ngakhale amene amatizunza , timakondwela ena a io akakhala Akristu oona . Lomba yelekezelani kuti mukuona angelo amene akukuuzani mofuula kuti : “ Usasoceletsedwe na mabodza a Satana ! ” Iye anati : “ Cinali covuta kusiya nyumba yathu yokongola na malo athu m’dela labwino . Pezani cimwemwe mwa kuwonjezela luso pa nchito . 65 : 22 . Ena makolo ao anamwalila cifukwa ca matenda , ngozi kapena tsoka linalake . M’mabanja ambili , ana amene akhala pafupi ndi makolo ndiye amapeleka cisamalilo cacikulu . N’cifukwa ciani tifunika kuyamikila kuti tili ndi cikumbumtima ? Analinso kupeza nthawi yambili yoceza nao . Kodi Pali Vuto Ngati Munthu Atakhala Kuti Sali M’chipembedzo Chilichonse ? “ Cikondi sicicita nsanje , ” cotelo cikondi ceniceni sicimakhumbila zinthu kapena maudindo a ena . Mboni za Yehova mamiliyoni padziko lonse zimayesetsa kucita zimene zaphunzila m’Baibulo . Iye amaona kuti palibe aliyense angamuuze zocita , kuphatikizapo Akristu anzake , akulu , ngakhale gulu la Mulungu . Mwacitsanzo , m’bale angakonzekele bwino nkhani ndi kukaikamba bwino pa msonkhano waukulu . Polinganiza cikhulupililo na cikondi , Paulo analemba kuti : “ Ngati ndili ndi cikhulupililo conse coti n’kusuntha naco mapili , koma ndilibe cikondi , sindili kanthu . ” ( 1 Akor . Timacita zimenezi mwa kuthandiza anzathu kuona mmene ‘ Malemba amatithandizila kupilila . ’ Iye adzakukumbutsani mmene ndimacitila zinthu potumikila Khiristu Yesu , monga mmenenso ineyo ndikuphunzitsila kulikonse , mumpingo uliwonse . ” ( 1 Akor . Mwina ndi koyamba kuyenda ndi munthu amene muli naye mu ulaliki . ▪ Imfa , Mdani Wotsilizila , Idzaonongedwa Arthur anati : “ N’nali kumvetsela nkhani mwachelu . ” Kodi mtima wonyalanyaza malamulo a Mulungu umene Solomo anali nawo unabweletsa mavuto anji ? Iwo anali ocokela ku malo osiyanasiyana , anali ndi zikhalidwe zosiyana ndipo anali kukonda zinthu zosiyana . Iwo anayamba kukonda kwambili phunzilo la banja , ndipo tinali kuwalola kufotokoza maganizo awo momasuka . Mwa kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova Mulungu , ndapeza Atate wabwino koposa . Pamene munadziŵa kuti iye anapeleka nsembe ya dipo la Yesu , munayamba kukhulupilila nsembeyo ndi kukhala pa ubwenzi ndi Mulungu . 20 : 20 ) Nditapita nao kwa nthawi yoyamba , ndinawapempha ngati angandipatse gawo langalanga . Magaziniyi inati : “ Sitimatsutsa ngati Malemba akamba kuti munthu winawake , cocitika cinacake , kapena cinthu cinacake , cimaimila cinthu cina mtsogolo . Kaya ndiye cinali cifukwa cake kapena ayi , mfundo ni yakuti anaponyedwa m’ndende popanda colakwa . Anthu amaganizila kuti nkhani ya m’nthano imeneyi inacitika kale kwambili uthenga wonena za Kristu usanafike ku mudzi kwa mtsikanayu . Takuya anakamba kuti : “ N’nali kucita mantha ndi manyazi nikafuna kuwatumila foni , koma nikawatumila , n’nali kulimbikitsidwa . ” ( Salimo 83 : 18 ; Mateyu 6 : 9 ) N’naphunzila kuti Yehova Mulungu amapatsa anthu onse ciyembekezo cokhala m’paradaiso padziko lapansi kosatha . M’nkhani ino , taphunzila mmene kusinkha - sinkha malonjezo a Mulungu na kupemphela nthawi zonse kungalimbitsile cikhulupililo cathu . Mau a Paulo olembedwa pa 2 Timoteyo 2 : 19 amachula za maziko . Ndipo maziko amenewo ali ndi cidindo ca uthenga . Kodi iye akuganizila ciani ? Nanga akumvela bwanji ? Tidziŵa kuti Yehova safuna cabe kutigwilitsila nchito panopa ndi kutisiya pambuyo pake . ” ( Sal . Kodi mabuku ouzilidwa amene mtumwi Yohane analemba alimbikitsa bwanji Akhristu kwa zaka zambili ? Kodi mapeto ali pafupi ? M’nkhani ziŵilizi tidzakambilana za mafumu anayi aciyuda ndi zolakwa zimene anacita . Zina mwa zolakwa zawo zinali zazikulu . Cinanso , kuphunzila Baibo kudzakuthandizani kudziŵa zinthu zina zimene mufunika kuwongolela potumikila Mulungu . 8 : 20 - 23 . Cifukwa ca mau amenewa , n’naganiza zocoka . Mofananamo , kudziŵa Mulungu kupitila m’Baibulo , kwathandiza anthu mamiliyoni ambili padziko lonse kusintha umoyo wao . ( Salimo 94 : 19 ) Kukamba zoona , timapindula m’njila zambili ngati tiŵelenga ndi kusinkhasinkha Malemba tsiku lililonse . — Machitidwe 17 : 11 . Kuti akwanitse kugwila nchito imene anapatsiwa , ophunzila a Yesu anafunika kugonjetsa khalidwe la kunyada na tsankho . ( Salimo 37 : 29 ) Anthu okhulupilika “ adzasangalala ndi mtendele woculuka . ” ( Afilipi 4 : 5 ; 1 Petulo 4 : 7 ) Ngati akulu ndi zitsanzo zabwino “ kwa gulu la nkhosa , ” tingaphunzile kwa io ndi ‘ kutsanzila cikhulupililo cao . ’ — 1 Petulo 5 : 3 ; Aheberi 13 : 7 . Cifukwa ca cikhulupililo cake , mkaziyo anacilikiza makonzedwe a kulambila koona apanthawiyo . Timalimbikitsidwa mapemphelo athu akayankhidwa “ Ndipo Yehova anamuuza kuti [ Solomo ] : ‘ Ndamva pemphelo lako ndi pempho lako lopempha cifundo kwa ine . ’ ” — 1 Mafumu 9 : 3 . Phunzilani citundu cawo ndi cikhalidwe cawo . Inde , anthu kulikonse padzikoli amalakalaka kukhala na ufulu wocita zilizonse zimene afuna na kukhala na umoyo mmene afunila . ( Machitidwe 16 : 10 - 12 ; 20 : 5 , 6 ; Akolose 4 : 14 ) Iye ayenela kuti anali kuthandiza Paulo ndi anzake akadwala pamaulendo aumishonale . Timamuonetsanso funso lofunika kudzakambilana ulendo wotsatila . — 8 / 15 , tsamba 13 - 14 . Ndipo ndimayamikila udindo wa Yesu pondithandiza kum’dziŵa bwino Mulungu . Zimenezi zandilimbikitsa kwambili . ” KUONONGEDWA KWA ANTHU AMENE AMAKONDA ZA DZIKOLI . Yerusalemu atatsala pang’ono kuonongedwa , Baruki anayamba ‘ kufunafuna zinthu zazikulu . ’ Adzakulimbitsani ndi kukupatsani mphamvu . ” — 1 Pet . Tinali kukhulupilila zimenezi cifukwa buku la Chivumbulutso limanena kuti Satana Mdyelekezi adzatsogolela anthu amene adzaukila anthu a Mulungu . ( Chiv . Nanga zipatso zimene tifunika kubala n’ciani ? ( 1 Pet . 1 : 24 , 25 ) Conco , tifunika kumaŵelenga Mau a Mulungu nthawi zonse , kuwaseŵenzetsa mu umoyo wathu ndi pophunzitsa ena . Nthawi zambili tikapita paulendo monga banja , makolo anga ayenela kuti anali kukhumudwa cifukwa ndikakhala pampando wakumbuyo mu galimoto , ndinali kuŵelenga buku mmalo moyang’ana cilengedwe panja . Kukonda kuŵelenga kunandithandiza kwambili pa maphunzilo a kusukulu . Anakambanso kuti anthu adzakhala osakhulupilika . ( Yer . 9 : 24 ) Mulungu sadalila buku lililonse la malamulo opangidwa ndi anthu opanda ungwilo kuti adziŵe cimene cili colungama ndi coyenela . Mavesi otsatila palembali aonetsa kuti pali kugwilizana pakati pa mmene timagwilitsila nchito “ cuma cosalungama , ” ndi kukhala okhulupilika kwa Mulungu . Koma anadziŵa kuti Mulungu ali ndi mphamvu zomuukitsa kwa akufa . M’bale wina wa ku Tokmok anatiitanila ku phwando la cikwati . Ndipo mu mlalang’amba uliwonse muli nyenyezi mabiliyoni ambili ndi mapulaneti . Ngakhale kuti Yesu sanakambepo zakuti mbalame zimakhala ndi malo okhala , Yehova anazilenga ndi nzelu ndiponso luso ndipo amazipatsa zinthu zofunikila kuti zikwanitse kumanga zisa zokhalamo . Maganizo anga oipa anayamba kucoka pang’ono - pang’ono . Nsanje yao inawasonkhezela kucita zinthu zimene patsogolo pake anadzacita nazo cisoni . N’nakhala waciwawa . Kambani ndi Mboni za Yehova za kwanuko . ( Yesaya 46 : 10 ) Kodi zimene Mulungu amanena zimacitikadi ? Anadzipeleka ku Taiwan , 10 / 15 Kodi kukhala wacifundo kumatanthauza ciani ? ( Gen . 35 : 10 , 22b - 26 ) M’kupita kwa nthawi , ana amenewa anakhala atsogoleli a mafuko 12 a Isiraeli . ( Maliko 14 : 22 - 24 ) Conco , n’zoonekelatu kuti mkate ndi vinyo ndi ziphiphilitso kapena zizindikilo . ( Salimo 145 : 19 ) Koma kodi Mulungu amayankha bwanji tikamupempha kuti atipatse mphamvu zotithandiza kupilila ? 20 : 28 - 30 ) Aja amene anali akulu kale koma apitiliza kutumikila Mulungu mosangalala monga ofalitsa , amaonetsa kwa onse , kuphatikizapo Satana , kuti cikondi cao pa Yehova ndi ceniceni . ( Tito 2 : 3 - 5 ; Yakobo 5 : 13 - 15 ) Komabe , sitiyenela kuuza munthuyo kuti atipangile cosankha . ( Aroma 5 : 12 ) Cifukwa cokana kutsogoleledwa na Mulungu , iwo anataya ufulu weni - weni umene anali nawo poyamba . Pamene tinatsegula citseko , tinawaona eni nyumbayo ataimilila pa pakhomo ali na cimpeni m’manja . Kwa zaka zambili , angelo akhala akuthandiza anthu okhulupilika Bodza imawononga onse aŵili , wonamayo komanso wonamizidwa . ( Yoh . NYIMBO : 68 , 72 Kuononga dzila limene layamba kale kukhala kamwana kuli ngati kucotsa mimba . Pa tsiku la 7 , asilikaliwo anazungulila mzindawo nthawi zokwana 7 . Nkhani iyi idzafotokoza mmene tingaseŵenzetsele cuma cathu kuti ‘ tidzipezele mabwenzi ’ kumwamba . Kukhala Wogontha Sikunanilepheletse Kuphunzitsa Ena ( W . ( Mat . 24 : 14 ) Yesu anali kulamulila kumwamba ndipo anali atasonkhanitsa kagulu kocepa ka atumiki ake oyeletsedwa padziko lapansi . Iwo asankha iwe kuti nikuyendele . ” Pamene ananitsekela m’maselo nekhanekha n’nacita mantha kwambili . Ngati tilephela kukhululukila ena , Atate wathu angacititse mphamvu ya nsembe ya Mwana wake kuleka kugwila nchito kwa ife . ( Mat . Conco , cinamuŵaŵa kuona kuti iwo anakana cifundo ca Mulungu . Monga Akristu colinga cathu ndi kukhala ‘ olumikizika bwino ndi ogwilizana , ’ kutanthauza kugwilila nchito pamodzi mogwilizana . Kodi Akhiristu akumanapo na zilizonse zolingana na ukapolo wa Ayuda ku Babulo ? Ai , sizitanthauza zimenezo . 3 Kukambilatu Zakutsogolo ( Ŵelengani Miyambo 6 : 16 - 19 ; Chiv . Kodi mungamvele bwanji ngati mnzanu wapamtima wakulekelelani pamene mwakumana ndi vuto lalikulu ? Ndiye cifukwa cake timanena kuti misonkhano yathu imakhala yosangalatsa caka ciliconse . Ndithudi , tonse tiyenela kuyesetsa kumaganizila zofuna za ena . Tiyenela ‘ kumatonthozana mwacikondi , ’ kuonetsa “ mzimu woganizilana , ” komanso kusonyeza ‘ cikondi cacikulu ndi cifundo ’ kuti tilimbikitse abale na alongo athu . Ngakhale kuti ndinapeza mfundo zina zosangalatsa , sindinakhutile . Mau akuti “ bungwe lolamulila ” anayamba kuonekela m’zofalitsa zathu ca m’ma 1940 . Panthawi imeneyo , zinali kuoneka kuti bungwe lolamulila linali kugwilizana kwambili ndi Watch Tower Bible and Tract Society . ( Ŵelengani Luka 2 : 41 - 47 . ) NYIMBO : 28 , 32 Conco , tinayembekezela kwa nthawi yaitali yankho yocoka ku Beteli , koma tinali kungopeza kuti m’bokosi ya makalata mulibe ciliconse . Ndipo kumvetsela mwachelu nkhani ya Cikumbutso kudzakuthandizani kukonda anansi anu ndi kuwauzako zimene mwaphunzila ponena za cikondi ca Yehova ndi colinga cake ponena za anthu . ( Mat . Koma Yosefe anali kudziŵa . Tafotokoza zocitika zitatu zosonyeza mmene Mulungu analoselela zinthu zamtsogolo mwatsatanetsatane . Pamafunika cikondi ndi kulimba mtima kuti tithandize munthu wocimwa . Davide sanadziyelekezele ndi Goliyati . Kodi zimenezi ziyenela kutidetsa nkhawa ? Iye anaonetsa khalidwe la kudziletsa pamene anali kutumikila m’nyumba ya Potifara , mkulu wa asilikali olondela mfumu Farao . N’cifukwa ciani kukambilana zifukwa zimenezo n’kofunika ? Tidzakambilananso cifukwa cake n’zotheka munthu kusintha ngakhale kuti analoŵelela kwambili m’makhalidwe oipa . Kodi tiyenela kuyesetsa kucita ciani ? Nchito imene iye anali kucita inali yofunika kwambili . Panthawiyo , anthu anali pafupi kwambili na ungwilo umene Adamu na Hava anataya . Kodi kumvela malangizo amene timapatsidwa masiku ano kungatithandize bwanji kukonzekela dziko la tsopano ? Mboni zina zocokela m’maiko ena zinapezekapo . 7 , 8 . ( a ) Ndi mfundo zina ziti zimene tikuphunzila m’fanizo la Yesu la wofesa mbeu amene amagona ? Iwo anacita zimenezi kuti adzauke kwa akufa , komwe ndi kuuka kwabwino kwambili . ” ( Aheb . Iye amakhulupilila kuti “ dziko likupita limodzi ndi cilakolako cake , koma wocita cifunilo ca Mulungu adzakhala kosatha . ” Conco , n’nadziŵa kuculuka kwa zinenelo zimene magazini athu anali kupulintiwa ku Brooklyn ndi kutumizidwa m’maiko ena padziko lapansi . Komabe , zocitika zionetsa kuti mkati mwa zaka zambili zokafikitsa ku nkhondo yoyamba ya dziko lonse , atumiki a Mulungu odzozedwa anali kumasuka mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu , osati kuloŵamo yayi . Fanizo limeneli limatanthauzanso uthenga wa Ufumu ndi zotsatilapo za nchitoyo . Koma kupemphela ndi kuŵelenga Baibulo kumandithandiza kuti ndigone . “ Madokotala ambili anam’cititsa kumva zopweteka zambili . N’nazindikila kuti cimene cinganithandize kusintha khalidwe langa ndi kupewa anthu amene anali kunisonkhezela kucita zoipa . Ngakhale lomba , ofalitsa pafupi - fupi 1,000,000 a ku Mexico akali nawo mzimu woyamikila zinthu zauzimu . Koma nthawi zina zocita za munthu zingapangitse ena kulephela kum’patsa malangizo a m’Malemba . Malemba amakamba kuti anthu ocimwa amene amathaŵila kwa Yehova , safunika kumangodziimba mlandu . Hezekiya “ anacotsa malo okwezeka , kugwetsa zipilala zopatulika , ndi kudula mzati wopatulika . Tengelani citsanzo ca Yesu : Phunzilani pa citsanzo ca Yesu ca mmene anali kuphunzitsila ophunzila ake . Yesu anauza omvela ake kuti : “ Samalani kuti musamacite cilungamo canu pamaso pa anthu ndi colinga cakuti akuoneni . . . muja amacitila onyenga . ” Izi n’zimene Satana amafuna kuti mtumiki wa Mulungu acite akakumana na mavuto . Kukumbukila zimenezi kuyenela kuti kunalimbikitsa Paulo kukhulupilila kuti Yehova adzamuthandiza kupilila mavuto amene anali kukumana nao , ndiponso amene akanakumana nao mtsogolo . Mfundoyi inali kulimbikitsa kwambili anthu kuti azilankhula zoona . Anthu akafuna kugwa , amagwila cinacake . Ŵelengani Aefeso 4 : 26 . Pa msonkhano umenewo acicepele onse kuphatikizapo Shannon ndi mng’ono wake anapemphedwa kuti akhale pamalo ena ake apadela . N’cifukwa ciani Yesu anacha nkhosa kuti ‘ olungama ’ ? ( Machitidwe 19 : 19 , 20 ) Mofananamo , kuti Mulungu akutetezeni , muyenela kuwononga zonse zokhudzana na ziŵanda monga zithumwa , mabuku a zamatsenga , na mankhwala otsilikila . ( Aroma 15 : 7 ) Iye anachula maina a abale amene anali ‘ kumulimbikitsa . ’ 25 : 2 ; 2 Akor . Ngakhale kuti sicinali copepuka , io anacita zonse zotheka kuti apitilize kusonkhana . Sin’nali kudziŵa kuti coonadi camtengo wapatali cokamba za Yehova Mulungu na colinga cake cidzasintha kwambili umoyo wanga . Bukulo linakambanso kuti io akapeza anthu anjala , osungulumwa , ndi odwala , amawathandiza , koma saiŵala kuti colinga cao cacikulu ndi kulalikila za kutha kwa dzikoli ndi kuphunzitsa anthu za cipulumutso . ( 2 Akor . 1 : 8 ; 7 : 5 ) Pamene Paulo anaganizila za moyo wake ndi mavuto ambili amene iye anakumana nao monga Mkristu wokhulupilika , iye anati : “ Ndani ali wofooka , ine osakhalanso wofooka ? ” Atsuko , mlongo wokwatiwa wa zaka za m’ma 30 wocokela ku Japan , anati : “ Kale , n’nali kungofuna Aramagedo itabwela mwamsanga . Pafupi ndi nyumba yaciŵiliyi panali munda wa mpesa . Kodi Abulahamu anaonetsa bwanji kuti anali kukhulupilila kuti Yehova amacita zinthu mwacilungamo ? 4 : 23 , 24 ) Popeza kuti ndise opanda ungwilo , tonse tifunika kupitiliza kuwongolela zimene siticita bwino . 1 : 7 , 8 . Tiyeni tikambilane za ciyambi ca cikwati na cifuno cake kuti tikhale na kaonedwe kabwino ka mgwilizano umenewu , ndi kutinso tione madalitso ake . Popeza n’zotheka ‘ kulola ’ kapena kuletsa ucimo kutilamulila , funso n’lakuti , Kodi mtima wanga udzasankha citi maka - maka ? Ndiyeno , m’kupita kwa nthawi kambilanani naye malemba ena ndi kumuthandiza kuganizila kwambili za kudzipeleka kwake kwa Yehova . ( Mlal . 5 : 4 ; Yes . 6 : 8 ; Mat . 6 : 24 , 33 ; Luka 9 : 57 - 62 ; 1 Akor . 15 : 58 ; 2 Akor . 10 : 4 , 5 . 25 : 21 , 23 , 34 . Iye anali kutumikila ku Bolivia akalibe kuyenda ku Ghana . Pofuna kuonetsa kuti anali ndi cikhulupililo cacikulu mwa Yesu , maiyo anayankha kuti : “ Inde Ambuye , komatu tiagalu timadya nyenyeswa zakugwa patebulo la ambuye ao ” Yesu anacita mogwilizana ndi pempho la mayiyo , ndipo anacilitsa mwana wake . — Mat . Aka n’koyamba akatswili ofukula zinthu zakale kupeza dzina limeneli m’zolemba zakale . Solomo mwana wa Davide atayamba kulamulila , anapempha nzelu kwa Mulungu ndipo anapatsidwa nzelu zoculuka . Tikamacita zimene timakhulupilila m’pamene timaona ubwino wokhala wosiyana ndi anzathu . ” Cikumbumtima canu cophunzitsidwa bwino cingakuthandizeni kupewa mavuto ( Onani ndime 14 ) 18 Fufuzani Cinthu Camtengo Wapatali Kuposa Golide Mkhristu waconco amalola maganizo ake kutsogoleledwa na mzimu woyela . ( Onani cithunzi - thunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) Coonadi ca m’Baibulo Cinandithandiza Kupeza Mayankho Okhutilitsa 8 N’tayamba kuwaŵelenga , n’nacita cidwi kwambili na zithunzi zake zokongola . Komiti ya Utumiki Kumbali ina , kuli Yehova , Mfumu yathu Yesu Kristu , odzozedwa amene anaukitsidwa , ndiponso angelo ambilimbili . Mkazi ali ndi udindo wapamwamba wokhala “ mnzake ” wa mwamuna . Koma tiyenela kuyesa - yesa mofanana ndi Paulo . Aroma caputa 8 imasiyanitsa anthu amene amayenda “ motsatila zofuna za thupi ” ndi amene amayenda “ motsatila za mzimu . ” Tinayamba kutumikila pa nthambi ya ku Brooklyn mu July 1990 . Iye anakamba zoona ngakhale kuti anadziŵa kuti Khoti Lalikulu la Ayuda lingamuimbe mlandu wonyoza Mulungu , ndi kuti zimenezi zingacititse kuti aphedwe . — Mateyu 26 : 63 - 67 . Seŵelo la “ Eureka X ” la mau okha linali kuulutsidwa masana kapena usiku . Mtsikana wina dzina lake Heather anati : “ Kupanga zosankha n’kovutadi . 10 : 22 ) Patapita zaka zambili , io ayenela kuti anali kusangalala kuona kuti zinthu zimene anapanga zikugwilabe nchito mu utumiki wa Yehova . Tifunika kucita zimene tasankha . Iwo angamalakelake kuona ana ndi adzukulu awo kaŵili - kaŵili . N’cifukwa ciani nthawi zina Mulungu sangacitepo kanthu ngati takhumudwitsidwa ? Kodi ndimapatula nthawi yocita Kulambila kwa Pabanja mlungu uliwonse ? ’ Nanga n’cifukwa ciani zimenezi n’zocititsa cidwi ? 1 : 9 . ( Rute 1 : 16 , 17 ) Kuŵelenga buku la m’Baibulo lochedwa ndi dzina la Mfumukazi Esitere ndi nkhani zina za iye , kudzalimbitsa cikhulupililo cathu . Paulo analangiza Akristu odzozedwa kuti ayenela kuika maganizo ao pa kukhala nzika zakumwamba osati pa zinthu za dziko lapansi . ( Afil . Kapenanso muona kuti pali nkhani ina yake imene sakukuuzani . Ndiyeno anawonjezelanso kuti : “ Umutulile Yehova nkhawa zako , ndipo iye adzakucilikiza . ” Mosasamala kanthu za mmene munakulila , mungavomeleze kuti Rabeka anali kupita kumalo amene sanali kudziŵa . Komabe , zingakhale bwino kuganizila nkhaniyo mwapemphelo ndi kuona ngati makolo ao afunikiladi zimenezo . Kodi tingaonetse bwanji kuti timayamikila zinthu zonse zimene Yehova ndi Yesu aticitila ndiponso zimene adzaticitila mtsogolo ? ( Gen . 3 : 1 - 5 ) Cinanso , iye anaonetsa kuti palibe munthu amene ni wokhulupilika kwa Mulungu ndi mtima wonse , ndi kuti aliyense angakane ulamulilo wa Yehova ngati atakumana ndi mavuto aakulu . ( Maliko 13 : 10 ) Popeza kuti nchito yolalikila ni yofunika kugwilidwa mwamsanga , tiyenela kuiona kukhala cimodzi mwa zinthu zofunika kwambili mu umoyo wathu . Koma kodi cimwemwe cimene amapeza cimakhala cokhalitsa ? Pamene tithandizila “ munthu wonyozeka , ” timatsatila citsanzo ca Yehova , ndipo timam’kondweletsa . ( Sal . 41 : 1 ; Aef . Nkhawa zina zingabwele cifukwa ca zolakwa zimene munthu anacita kumbuyoku . Zekariya na Ayuda anzake anali kudziŵa kuti ku Sinara , kapena kuti ku Babulo , kunali kucitika zoipa zambili m’nthawi yawo . 2 : 15 ) Timayesetsa kukana zoipa . ( Yak . Njila yokha imene io akanawolokela mtsinjewo ndi mwa kuponda pa miyala ikulu - ikulu imene inali pamtsinjewo . Akakamba kuti adzacita cina cake , cili monga kuti wacita kale cinthuco . Masomphenya amenewa onena za Mulungu , agwilizana na mau amene wamasalimo analemba akuti : “ Pakuti Yehova ndi wamkulu ndi woyenela kutamandidwa kwambili . ( Aroma 5 : 8 , 12 ; 6 : 23 ) Conco , Mulungu woona Yehova , anatuma Mwana wake Yesu padziko lapansi kuti adzapeleke moyo wake ndi kuombola moyo umene Adamu anataya . — Ŵelengani Yohane 3 : 16 . Ngakhale n’conco , panthawi zina anacita macimo akulu - akulu . Ndiyeno , timayesetsa kupatula nthawi yokwanila yoceza na abale na alongo . ” Popeza anatilenga ndi ufulu wodzisankhila zocita , iye amalemekeza ufulu ndi udindo wathu ‘ wosankha ’ tokha kum’tumikila kapena ayi . ( Yos . 24 : 15 ; Mlal . Mudzaphunzilanso za maphunzilo othandiza amene ofalitsa Ufumu akhala akulandila kwa zaka zambili . Masiku anonso anthu akhala akufufuza njila zothetsela imfa . Niyembekezela mwacidwi nthawi imene tidzaonananso . Debora ndi Baraki anayamikila “ atsogoleli a asilikali a Isiraeli amene anadzipeleka mwaufulu pakati pa anthu awo . ” A MBONI za Yehova ambili masiku ano akulalikila mwacangu . Iwo akukwanilitsa ulosi wakuti uthenga wabwino udzalalikidwa “ kudziko lililonse , fuko lililonse , cinenelo ciliconse , ndi mtundu uliwonse . ” ( Chiv . Iwo pamodzi na Yesu adzalamulila anthu monga mafumu . Conco , ndinafunika kusankha kupita kapena ai . Kodi Yesu ali ndi mbali yotani pa kukwanilitsa cifunilo ca Yehova ? ( a ) Tingaphunzile ciani m’fanizo la Yesu la mpesa ndi la wofesa mbewu ? Kaya tingakwanitse kusamukila ku malo osoŵa kapena ai , tonse tiyenela kucita zimene tingathe kuti tithandize ena mumpingo wathu . Ganizilani izi : Kuti munthu akwanitse kukwela Phili lalitali kwambili , amafunika kudya cakudya cimene akanadya kwa masiku atatu kapena anai . Nkhani zina zimafunika kuzifotokozanso mwa njila ina . ” Iye anati : “ Munamva kuti anthu akale anauzidwa kuti , ‘ Usamalumbile koma osacita , m’malomwake uzikwanilitsa malonjezo ako kwa Yehova . ’ ” — Mat . Kale , nthawi zina Yehova anali kucita zozizwitsa pofuna kuonetsa kuti anthu ake amawayanja . Kodi mungaciteko upainiya ? Nayenso Mlongo E . Kodi imwe mumaona kuti cilango cimene Mulungu amatipatsa kupitila m’Mau ake , zofalitsa , makolo acikhristu , kapena akulu mu mpingo , ni umboni wakuti iye amatikonda ? Baibulo limanena kuti : “ Anthu onse a ku Yuda anali ataimilila pamaso pa Yehova , kuphatikizaponso akazi ao ndi ana ao , ngakhalenso ana ao ang’onoang’ono . ” Kodi zikumbumtima zingasiyane bwanji ? Pambuyo pake , munthu aliyense amene adzapandukila ulamulilo wa Mulungu adzaonongedwa nthawi imeneyo . Loyamba ndi Chivumbulutso 12 : 10 , 11 , limene limanena kuti Mdyelekezi anagonjetsedwa osati cabe cifukwa ca mau athu a umboni komanso cifukwa ca magazi a Mwanawankhosa . ( a ) Ndi ndandanda yotani imene Mkristu wofikapo amakhala nayo ? Baibulo limanena mosapita mbali kuti Aisiraeli sanazengeleze pamene anauzidwa kuti ‘ acoke kumahema a Kora , Datani , ndi Abiramu . ’ Kodi kupanduka kwa mu Edeni kwawakhudza bwanji amuna ndi akazi ? Tiyeni tikambilane ziŵili cabe . Munayamba mwadzifunsapo kuti ‘ Kodi kumwamba n’kwabwanji nanga kumakhala ndani ? ’ Tifunika kuphunzila Baibulo nthawi zonse , kusinkhasinkha pa zimene taŵelenga , ndi kupempha Yehova kuti atithandize kugwilitsila nchito zimene taphunzila . Ngakhale kuti mwina munakhala Mboni caposacedwapa , kodi mumaika maganizo anu pa ciani ? N’cifukwa ciani tifunika kukhala ndi cikumbumtima cabwino ndi codalilika ? 30 Mungacite Ciani Kuti Mujaile mu Mpingo Wanu Watsopano ? N’cifukwa Ciani Kudzicepetsa N’kofunikabe ? Jan . Cifukwa Baibo ili na malangizo othandiza kupewa nkhawa , kuzicepetsa , kapena kulimbana nazo . TSAMBA 27 • NYIMBO : 89 , 135 ( Mlaliki 12 : 1 ) Mau amenewa anam’thandiza kwambili Timoteyo atakhala Mkristu . Pambuyo pa zaka pafupi - fupi 400 Aisiraeli atatuluka mu Iguputo , io anapempha Mulungu kuti awapatse mfumu yaumunthu potengela mitundu ina . Kucita izi kudzawathandiza kupeza mabwenzi atsopano na kujaila umoyo wa m’delalo . ( Luka 22 : 20 ; ŵelengani Aheberi 9 : 15 . ) Motelo , ophunzila amenewa anapanga mtundu watsopano wa Yehova . Ine ndi mkazi wanga timakondwela ndi utumiki . Zosankha zimenezo n’zimene zidzaonetsa ngati timayesetsa kutengela maganizo a Khristu . Koma popeza kuti Mulungu ali ndi ‘ mphamvu zoopsa , ’ n’zosacita kufunsa kuti Ufumuwu udzapatsa nzika zake zinthu zoculuka zofunikila . — Yesaya 40 : 26 ; Salimo 145 : 16 . ( Ezara 3 : 12 ) Mukanakhalapo pa ulendowo , kodi mukanamvela bwanji kuona Yerusalemu , malo anu atsopano okhala ? 34 : 22 . Ngati tipeleka ulemu woyenelela kwa akulu , m’malo mowatamanda monga anthu ochuka a m’dzikoli , ndiye kuti tikuwathandiza . Nthawi yanga yogula itafika , ndinaona kuti ndi yogati . Iwo anati , “ Cimwemwe cimene timakhala naco pothandiza anthu odzicepetsa kudziŵa Yehova , sitingaciyelekezele na cina ciliconse . ” Yesu anacita zinthu mosamala kuti asatengeko mbali pa mikangano imeneyi ya misonkho . Kutengela zocita za ena kungaticititse kupanga zosankha zolakwika . ( a ) Kodi Yobu anacita ciani cimene cinaonetsa kuti anali wokhulupilika kwa Mulungu ? Conco , m’pomveka kuti “ ndodo ya Efuraimu ” inaimila mafuko 10 a ufumu wakumpoto . Ganizilani zimene mungacite kuti mucepetseko nthawi yogwila nchito ( Aheberi 12 : 2 ) Iye sanatengeke maganizo ndi zinthu za m’dzikoli . ( Luka 9 : 46 - 48 ) Ngati mwamuna atengela citsanzo ca Yesu , angakope mkazi wake kuti ayambe kutumikila Yehova . Alongowo anamuthandizadi . Inunso mukapilila ciyeso , ena adzalimbikitsidwa . Amene amakhulupilila dipo ya Khiristu , komanso amene amacita cifunilo ca Mulungu angakhale pakati pa anthu amene akufuula kuti : “ Cipulumutso cathu cacokela kwa Mulungu wathu , amene wakhala pampando wacifumu , ndi kwa Mwanawankhosa . ” — Chiv . Nthawi ina anaonekela kwa anthu oposa 500 . Kulandila thandizo pa nthawi yoyenela ( Onani ndime 13 ) Kodi na ise zaconco zingaticitikile ? Iye sanawole , koma ali kumwamba ndipo ali na moyo ‘ wamuyaya . ’ — Aroma 6 : 9 ; Chiv . Koma angelo opanduka amenewa sali gulu laciwawa lopanda dongosolo . ( b ) Kodi cofunika n’ciani kuti kuŵelenga Baibo kukhale kopindulitsa ? KUIKA ANTHU PATSOGOLO , ZINTHU PAMBUYO . Mwana wake ‘ analilila unamwali wake . ’ Ena amakhulupilila kuti anthu angakwanitse kuthetsa mavuto ngati acita zinthu mogwilizana . Pamene ena amaona kuti mavuto sangasile padziko . ( b ) Kodi ndi mafunso ati amene tifunika kuganizila ? MATEYU 14 : 23 Lolani Yehova Kulimbitsa ndi Kuteteza Cikwati Canu Kuti tikwanitse kucita nchito imeneyi , tamasulila ndi kufalitsa mabuku , magazini , tumapepala twauthenga , toitainila anthu ku Cikumbutso , ndi ku msonkhano wacigawo m’zinenelo zoposa 700 . Simon anati : “ Ukakhala mlendo ku dziko lina , zonse zimakhala zacilendo . Gehazi waumbombo anakanthidwa ndi khate la Namani . — 2 Maf . Ni vuto lanji limene linabuka pakati pa Aisiraeli cakumapeto kwa ulendo wawo wa zaka 40 wa m’cipululu ? ( Chivumbulutso 7 : 10 , 16 , 17 ) Yesu anakamba kuti : “ Bwelani kwa ine nonsenu ogwila nchito yolemetsa ndi olemedwa , ndipo ndidzakutsitsimutsani . Kuphunzila Malemba nthawi zonse m’cinenelo cathu , kudzatithandiza kukhalabe auzimu pamodzi na banja lathu . CIKONDI Onse anapita . Iye ndi mkazi wake ndi apainiya anthawi zonse ndipo amasamalila banja lalikulu . ( b ) Kodi Akhristu amene ali na nyumba zosaukila angapeleke malo awo kwa alendo ? 4 : 17 ) Citseko cidzatsekedwadi kuti osakhulupilikawo , amene adzakhala ngati anamwali opusa asaloŵe . Kwa akulu - akulu a chechi , cimeneci cinali cipanduko . Onani zimene Yehova adzaticitila . Pa mavuto . Makolo angalele bwino ana ao ngati akukondana ndi kulemekezana . Pewani kugula zinthu zosafunika kweni - kweni Magaleta na Cisoti Cacifumu Zimakutetezani , Oct . Popeza kuti Yosefe anali kufuna kuti bambo ake apitilize kumudalila , iye anapitilizabe kuvala mkanjo umene anamupatsa . 17 : 17 ) Mwacitsanzo , tingawathandize pa mavuto amene akukumana nao cifukwa ca ngozi yacilengedwe . Iye ndi wankhanza kwambili . Mtumwi Petulo ananenelatu kuti : “ M’masiku otsiliza kudzakhala onyodola amene azidzatsatila zilako - lako zao , amene azidzati : ‘ Kukhalapo kwake kolonjezedwa kuja kuli kuti ? Ngati tiganizila kwambili zinthu zoipa , cikhulupililo cathu cingayambe kufooka Ngati n’kotheka , pemphelani capamodzi . Koma umoyo masiku ano ndi ‘ wodzaza ndi mavuto ndi zopweteka . ’ ( Sal . Pocoka , mkulu wa apolisiyo anamwetulila ndi kutibayibitsa . ( a ) N’ciani cingathandize makolo kuona zinthu moyenela pokambilana ndi mwana nkhani yopalana cibwenzi ? Nthawi zina mwanayo angafunike kuyembekezela mpaka nthawi yoyenela itakwana . 13 : 34 , 35 . 26 : 31 - 33 ) Kudzidalila kwa Petulo kunali kosathandiza cifukwa usiku umenewo , iye analephela kuonetsa mzimu wodzimana . ( Aheb . 6 : 11 , 12 ; 10 : 24 , 25 ) Komanso , kuti akhale olimba mwauzimu , anali kugwilitsila nchito nthawi yawo mwanzelu . Mabwinja a nyumba zingapo amene anali pafupi ndi pamene panali kacisi apezeka ndi mabeseni osambilamo . Malaki anakamba kuti tiyenela ‘ kuopa Yehova ndi kuganizila za dzina lake . ’ 10 : 19 ; 17 : 27 ; Mat . 5 : 22 ) Ngati ena atikwiyitsa , tifunika ‘ kusiila malo mkwiyo . ’ “ Sitilinso acicepele amene savutika kuphunzila citundu , ” anatelo Nadine , kwinaku akumwetulila . Sindinali kuyembekezela kuti amai angakhumudwe nane , cifukwa cakuti ndinali kuwamvela nthawi zonse . Tisaleke kuyamikila mphatso yapadela imeneyi , mwa kuiseŵenzetsa polemekeza Mulungu , ndi mwa kulemekeza ufulu wa ena pa zosankha zawo . Mwacitsanzo , pa Filimoni 1 - 3 , Paulo anatumiza moni kwa abale onse mumpingo wa ku Kolose , ndipo ena anawachula maina . Timasonyeza kuti timakonda Mulungu ndi Mau ake mwa kuphunzila Baibulo mwakhama . Kumeneko tinaliko akaidi 300 , ndipo tinali kugona mopanikizana kwambili . Iye akanadziŵa zoopsa zimene adzakumana nazo , sakanayenda pafupi ndi nyumba ya mkaziyo . — Miy . 18 : 15 ) Yesaya anakambilatu kuti ameneyo adzakhala “ mtsogoleli ndi wolamulila . ” ( Yes . Ndipo funso lofunika kwambili n’lakuti , ni mfundo yanji imene tingatengepo pa cocitika cimeneci imene ingatithandize ngati mkulu wakamba kapena kucita zinthu zimene zatikhumudwitsa ? M’kupita kwa nthawi , mudzaona kuŵelenga Baibo kukhala kosavuta na kokondweletsa . Colinga cathu ndi kucita zinthu mogwilizana ndi mfundo za makhalidwe abwino a Yehova nthawi zonse . Eodiya ndi Suntuke ayenela kuti anali osiyana zibadwa , kapena anali osiyana m’njila zina . Umunthu wanu umaposa dzina lanu kapena maonekedwe anu . Kodi mumakonda kusankha mwekha zocita ? Kapena mumafuna anthu ena kukusankhilani ? 11 , 12 . ( a ) Kodi nkhani ya woyang’anila ndende igwilizana bwanji na nchito yathu yolalikila ? ( 2 Akor . 1 : 3 ) Yehova amakhudzika mtima pamene ticitila ena cifundo . Iye anaikanso “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” kuti azitsogolela pa nchito imene ikucitika m’mabwalo a padziko lapansi a kacisi wamkulu wauzimu . ( Mat . Yesu anatiphunzitsa kuti tifunika kukonda anzathu Anthu amafa cifukwa cokoka fodya . M’mau ena , Yehova akutiuza kuti tizitsatila Yesu ndi kuponda mapazi athu pamene iye anaponda . Ngakhale kuti Yesu anali wangwilo , iye nthawi zonse anali kulankhula ndi Yehova m’pemphelo . Kodi Yehova amaticenjeza , kutiongolela ndi kutitsogolela bwanji ? Ni madalitso anji amene timapeza ngati ticita zinthu mogwilizana na malamulo a Yehova na mfundo zake ? Iye amamvetsela mapemphelo athu onse mwachelu . Ngati tifuna kupanga cosankha cacikulu cimene cidzakhudza umoyo wathu ndipo m’Baibulo mulibe lamulo lokhudza nkhaniyo , tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi Yehova adzamva bwanji ndikasankha kucita zimenezi ? Cikhulupililo ceni - ceni cimacokela pa kum’dziŵa bwino Mulungu . Atamuona , Yesu anati : “ Onani Mwisiraeli ndithu , amene mwa iye mulibe cinyengo . ” ( a ) Polalikila tiyenela kukhala ndi ciani m’dzanja lathu ? N’ciani cimene tingacite kuti zaconco zisaticitikile ? Adani athu sadziŵa kapena kumvetsetsa cifukwa cake sititengamo mbali m’zinthu za dzikoli . 41 : 8 ; 55 : 6 ) Cifukwa ca zimene zinam’citikila wamasalimo , iye anati ponena za Yehova : “ Inu Wakumva pemphelo , anthu a mitundu yonse adzabwela kwa inu . Buku lina limati : “ Atsogoleli acipembedzo analimbikitsa anthu kumenya nkhondo m’malo mophunzitsa Baibulo . M’malo mwake , amasankha zipatso zonunkhila bwino , zokongola , zimene zangothyoledwa kumene , zakupsa bwino , ndi zokhwima . N’namuuza kuti n’nali n’tayamba kutsatila miyezo ya makhalidwe abwino ya m’Baibo . ( a ) N’ciani cimene Yesu anacenjeza ophunzila ake ? Simungadziŵe kuti kamodzi mwa tumapepa tumene tunatsalako , kangathandize munthu woona mtima kupezeka pa Cikumbutso . — Mat . Nthawi zonse nimayamikila Yehova cifukwa conipatsa mwayi wopezekapo . ’ ” 113 : 5 - 8 ) Davide anadziŵanso kuti zabwino zonse zimene anali nazo anapatsiwa na Yehova . — Yelekezelani na 1 Akorinto 4 : 7 . Muziimba Mosangalala ! Kwa zaka zambili , atumiki a Yehova anali kutsogoleledwa ndi mitu ya mabanja , imene inali kutumikila monga mafumu , oweluza , ndi ansembe . M’delali , Sara anali kukwanitsa kuona kukula kwa Dziko Lolonjezedwa . Ndiyeno anafotokozela Mariya kuti colinga ca Mulungu n’cakuti iye adzabeleke Mesiya . Manda akutenga anthu ambili . N’ciani cinacititsa mfumu yabwino imeneyi kucita zimenezi ? Mose anafunsa Yehova kuti : “ Ndine ndani ine kuti ndipite kwa Farao ndi kutulutsa ana a Isiraeli ku Iguputo ? ” ( b ) Kodi kuwawongolela kumeneko sikunatanthauze ciani ? Pangano la Ufumu linawatsimikizila kuti adzakhala pamipando yacifumu , ndi kulamulila monga mafumu ndi kutumikila monga ansembe . ( b ) N’cifukwa ciani acicepele angayambe kukaikila kulambila koona ? Kuti ticite zinthu mogwilizana ndi pempho lakuti “ mutilanditse kwa woipayo , ” tiyenela kuyesetsa “ kusakhala mbali ya dziko [ la Satana ] . ” Ku Sweden , aneba a mlongo Charlotte Ahlberg amene anasonkhana m’nyumba yake yaing’ono “ anakhudzika mtima kwambili ” atamva seŵelo la mau limeneli . Conco , anakamba mfundo yakeyo mwa fanizo , kuuza mayi wacigiriki kuti : “ Si bwino kutenga cakudya ca ana n’kuponyela tiagalu . ” 7 : 5 , 9 . 4 : 16 , 17 . Kuti nikhale na mtendele , n’nadziŵa kuti nifunika kusasunga cakukhosi . Ambili aona kuti kucita zambili potumikila Yehova akali acicepele , kwawathandiza kukhala na banja lacimwemwe . Koma Yehova anaphunzitsa anthu ake kuti sayenela kukhala ouma mtima mwanjila imeneyi . Kodi cofunika kwambili ni kukhala wodziŵika kwa ndani ? N’cifukwa ciani Solomo anafunika kukhala wolimba mtima ? Nanga tingacite ciani kuti tipambane polimbana ndi mdani wathu woopsa ameneyu ? Sitiyenela kuwapempha kuti asaine m’buku kapena m’Baibulo lathu . Pokamba za bukuli , dikishonale yochedwa The Oxford Dictionary of the Christian Church ( ya mu 1997 ) inati : “ N’zosakayikitsa kuti buku lakuti ‘ Acts of Paul and Thecla ’ lili na mfundo zina zolondola zokhudza mbili yakale . ” ( Akol . 4 : 10 ) Conco , monga mmene zinalili kale , ifenso masiku ano sitiyenela kulola kuti kusiyana zibadwa kusokoneze mtendele . ( Machitidwe 9 : 15 ) Yehova anasankhanso anthu ena ndi kuwaumba kuti akhale ‘ ziwiya zolemekezeka . ’ Pa anthu amenewo panali ena amene kale anali kuledzela , kucita ciwelewele , ndi kuba . Kodi Yehova anateteza bwanji anthu ake akale ? Nanga masiku ano amawateteza bwanji anthu ake ? Kukambilana zimenezi kudzatithandiza kudzipenda na kuona mmene tingaonetsele cikondi cimene cimabweletsa cimwemwe ceni - ceni . Kodi odzozedwa agwilitsila nchito bwanji uthenga wa m’fanizo la Yesu la anamwali 10 ? 7 : 26 ) Conco , mkate wopanda cofufumitsa ndi umene timagwilitsilanso nchito pa Cikumbutso . ( Salimo 25 : 14 ) Tikamayesetsa kusintha umunthu wathu kuti tim’kondweletse , iye adzatithandiza kuti tipambane . Amuna amenewa amapita kwa otsalila a odzozedwa kuti akawacilikize pa nchito yao ndiponso kuti akapeze thandizo la kuuzimu . Vesi 19 imapitiliza kuti : “ Ndipo ndinaona cilombo , mafumu a dziko lapansi , ndi magulu ao ankhondo atasonkhana pamodzi kuti amenyane ndi wokwela pahatchi uja ndi gulu lake lankhondo . ” N’tayamba kugwilizana ndi Mboni za Yehova , makolo anga anakalipa kwambili . Anacita zimenezo kwa milungu ingapo . Pambuyo popitako mobwelezabweleza , tsiku lina anam’peza panyumba . Iye ndi wa Mboni za Yehova . N’cifukwa ciani mafunso ndi ofunika ? Pa August 31 , 1947 , n’nadzipatulila kwa Yehova na kubatizika . Komabe , acibululu ake sanamvetsetse cifukwa cimene iye anakanila kucita maphunzilo apamwamba kuti akapeze nchito yabwino . Kapena mumamvela monga mmene Ed anamvelela ? Tikamagwila nchito imeneyi mwakhama ndi kukhalabe omvela ndi okhulupilika kwa Yesu , iye adzatifupadi . — Mat . Mwacitsanzo , sitidziŵa “ nthawi yoikidwilatu ” ya cisautso cacikulu . Lemba la Yesaya 60 : 17 . ( Ŵelengani . ) linanenelatu za kusintha kocititsa cidwi kwa mbali ya padziko lapansi ya gulu la Yehova . ( b ) Nanga wamasalimo amawacha bwanji akazi amene amalengeza uthenga wabwino ? 3 , 4 . ( a ) Kodi Ayuda a m’nthawi ya Yesu anali kuyembekezela ciani ? Marilyn sanafune kusiya banja lake la mtengo wapatali ndi kusiya kucita zinthu za kuuzimu pamodzi ndi banja lake . Ngakhale ndi conco , iye amasangalala ndi umoyo . Ngati n’conco , mudzapindula kwambili kuganizila mfundo zina zimene mtumwi Paulo analemba m’buku la Aheberi . Nyambo ina yokopa kwambili imene Satana amaseŵenzetsa ni zamizimu . Kodi lemba la Oweruza 5 : 31 limafotokoza zinthu ziti zimene zidzacitika mtsogolo ? Nkhaniyo inali kukamba za Doegi amene amachulidwa m’Baibulo . Anthu ambili anacita cidwi ndi zinthu za m’Malemba zimene zinali kupezeka m’magaziniwo kuphatikizapo m’buku lochedwa Zeze wa Mulungu la m’Cipolishi . Anthu ambili adzaphedwa padziko lapansi . Komanso , zopeleka zathu zaufulu zimathandiza pa nchito yokonza na kumasulila mabuku na mavidiyo , nchito yothandiza okhudzidwa na masoka , ndi yomanga Nyumba za Ufumu zatsopano . Pamene anali mnyamata , anakhala kapolo wa mankhwala osokoneza ubongo . Polangiza Akhristu kuti ayenela kulimbikitsana , n’cifukwa ciani mtumwi Paulo anakamba kuti “ tiwonjezele kucita zimenezi ” ? ( 2 Akor . 13 : 5 ) Mwacitsanzo , wofalitsa wobatizika amene mwadala wakhala akupenyelela zamalisece ayenela kudzifunsa kuti , ‘ Kodi ndikuyesetsa kukhala woyela ? ’ Yamikani Yehova Ndipo Mudzadalitsidwa Tifunika kudalila Mulungu kuti tikhale olimba mtima , oleza mtima , ndiponso kuti tikhalebe ndi mtendele wa m’maganizo pamene tikulimbana ndi mavuto a tsiku ndi tsiku . Ndithudi , madalitso ake onse ndi oona ndipo “ saonjezelapo ululu . ” — Miy . 16 : 9 , 10 . ( Machitidwe 2 : 4 - 11 ) Kenako , gawo lao linakula ndipo anayamba kulalikila ngakhale kwa Asamariya . Ana anu akamakumvelani mukupempha Yehova kuti akuthandizeni kukhala olimba mtima kuti mulalikile anansi anu , kapena kupempha abwana anu kuti akuloleni kupita ku msonkhano wacigawo , adzadziŵa kuti mumadalila Yehova , ndipo naonso adzacita cimodzimodzi . N’ciani cimene amuna ndi akazi angacite kuti azilola Yehova kutsogolela banja lao ? Komanso bwanji ngati iye angabatizike , kenako n’kugwela m’chimo ? ’ Nditawatumila foni , Atate anandiyankha kuti , “ Ndi kumalo kwabwino kumene ufuna kupita . ” Cifukwa ciani ? Tiyeni ticite zilizonse zotheka kuti tikapindule mwa kupezekepo pa Cikumbutso ca pa March 31 , 2018 . Iye anapilila khalidwe loipa la mkulu wake , Esau , amene anali kufuna kumupha . Ena ali yakali - yakali kufalitsa uthenga wabwino m’magawo a cinenelo cina . ( Sal . Kujaila mu Mpingo Wanu Watsopano , Nov . 3 : 2 . Koma ana athu amatangwanika na kuphunzila mau atsopano oseŵenzetsa mu ulaliki . Ngati n’conco , mungafunse kuti , ‘ N’ciani cingathandize anthu ofedwa kupilila ? ’ Pemphani Yehova kuti akuthandizeni kukulitsa cikhumbo com’tumikila . Caciŵili , pewani kudziculukitsila zocita . Pamene Yoswa anali kumenyana ndi Aameleki , Mose , Aroni ndi Hura anaima pa phili limene linali capafupi . ( Sal . 37 : 25 ) Komabe , mau a Davide satanthauza kuti wolambila Mulungu sasoŵa zofunikila kapena kuti sadzasoŵapo . N’cifukwa ciani mneneli amene anali wodzicepetsa poyamba anamvelela wokalamba wacinyengo ameneyo ? Inde , tonsefe tili ndi zifukwa zabwino zotsatilila malangizo akuti , “ muthandize ofookawo . ” — Mac . Cinthu congoyelekezela ? Koma tifunika kuziyembekezela , ndipo pali pano tikhoza kukumana na mavuto ambili . Komabe , Paulo anati : “ Pamene tinali adani , tinayanjanitsidwa kwa Mulungu kudzela mu imfa ya Mwana wake . ” N’cifukwa ciani nthawi zina Yehova sayankha mapemphelo athu nthawi yomweyo ? Iye anali kuŵelenga Nsanja ya Mlonda , ndipo anali ndi Baibulo . Iwo amadziŵa kuti Yehova wadalitsa odzozedwa , ndipo amaona kuti ndi mwai kutumikila Mulungu pamodzi nao . 31 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi N’cimodzi - modzi na Akhiristu odzozedwa . Iwo anali kudziona “ ngati akufa ku ucimo koma amoyo kwa Mulungu mwa Khiristu Yesu . ” Pa cifukwa cimeneci , makolo ena amaseŵenzetsa mabuku , zomvetsela , na mavidiyo a zitundu zonse ziŵili . mu Nsanja ya Olonda ya October 1 , 2012 . Kodi kukwanilitsidwa kwa lemba la Yesaya 60 : 17 kumatipangitsa kutsimikiza za ciani ? ▪ Tumikilani Mulungu Mokhulupilika Panthawi ya “ Masautso Ambili ” Koma Barizilai sanavomele . Malemba amati : “ Onse anadya ndi kukhuta . ” Cofunika ndi kumvela cenjezo . Tam’funafuna ndipo watipatsa mpumulo pakati pa adani athu onse otizungulila . ” Brook na Hans Iye analonjeza Yehova kuti ngati adzamuthandiza kupambana nkhondo , adzapeleka “ nsembe yopseleza ” munthu woyambilila kutuluka m’nyumba yake kudzamulandila pobwela kucoka ku nkhondo . Ambili a ife timakhala ndi zocita zambili . ( Lev . 13 : 43 - 46 ) Sitikudziŵa zimene Yesu anali kuganiza kwenikweni , koma timadziŵa mmene anali kumvelela . Asayansi apeza kuti cimakhala copepuka kukumbukila cinthu ngati tikuciŵelenga mokweza . ( Deut . 6 : 7 ) Anna , mwana wamkulu wa Eduardo anati : “ Pamene atate anali kukhala kutali ndi ife ndinaona kuti sanali kundikonda . Zidzatheka Kuti Padzikoli Pakhale Mtendele ? ( Chivumbulutso 14 : 6 ) Ngakhale kuti masiku ano angelo sakamba na anthu mmene anali kucitila kale , amatsogolela alaliki uthenga wabwino kuti apeze anthu a mtima wabwino . Mungacite ciani kuti mudzapulumuke pamene dziko loipali lidzawonongedwa ? N’ciani cimene tikuphunzilapo tikaona mmene Yehova amakambila ndi anthu ? Natanayeli anali kuona anthu a ku Nazareti mosayenela . Koma Yesu anakambilana naye mwaubwenzi . 8 : 13 ) Conco , njila zina zimene timayeletsela dzina la Mulungu ni mwa kuliona kukhala lapadela kwambili kuposa maina ena onse , komanso kuthandiza anthu ena kuti aziliona mwanjila imeneyi . Timaona zimenezi mwa mau a Paulo m’kalata yake asanalembe mau a m’caputa 8 . Mateyu caputa 4 , 10 , 14 , 16 - 17 , 26 ; Machitidwe caputa 1 - 5 , 8 - 12 Zikakhala conco , muyenela kupemphela kwa Mulungu ngati mmene Asa anacitila . Ndipo ngati acititsa phunzilo laconco , angacite bwino kumaphunzilila panyumba pa anawo pamodzi na makolo awo , kapena ali na Mkhristu wina wokhwima mwauzimu , kapenanso atakhala pa malo oonekela bwino . Panthawiyo , nkhondo yoyamba ya dziko lonse inali itafika poipa . Motelo , anaitanidwa kuti aloŵe usilikali . ( 2 Mbiri 32 : 25 , 26 ) Ngakhale kuti amunawa anali ndi zifooko , Aisiraeli anafunikabe kutsatila citsogozo cawo . 8 : 25 ) Kenako Yesu akuuka ndi kulamula mphepo ndi nyanjayo kuti : “ Leka ! Kodi Hezekiya anakulila m’banja lotani ? Nimapewa kuwaweluza . Ndipo anasunga pangano lao lakuti : “ Yehova akhale pakati pa iwe ndi ine , ndi pakati pa ana ako ndi ana anga mpaka kalekale . ” — 1 Samueli 20 : 42 . “ Nthawi zonse tikamakupemphelelani , timayamika Mulungu , Atate wa Ambuye wathu Yesu Khiristu . ” — Akolose 1 : 3 . N’cifukwa ciani okwatilana afunika citsogozo ndi citetezo ca Yehova ? Ndipo monga timaonela m’vikwati vambili masiku ano , amuna amacitila nkhanza azikazi awo . ( Gen . Mau a Mulungu amatikumbutsa kuti ‘ nzelu yocokela kumwamba ni yamtendele ndi yololela . ’ Buku ina inati : “ Ni mwa apa na apo pamene mau ena okayikitsa anawonjezeledwa kapena kucotsedwa . ” — The Book . Mdyelekezi analonjeza Yesu kuti adzamupatsa maufumu a dziko ndi ulemelelo wao ngati atamugwadila , koma iye anakana . ( Mateyu 12 : 13 ; Luka 22 : 50 , 51 ) Malonjezo a Yehova na zozizwitsa zimene Yesu anacita zimanicititsa kukhala wotsimikiza kuti posacedwa nidzakhala na ziwalo zonse . Ngati sitimvetsetsa Mau a Mulungu m’cinenelo cacilendo , umoyo wathu wa kuuzimu ungakhale paciswe . Kodi zidzatheka kuti padziko lapansi pakhale cilungamo ceni - ceni ? Afunikanso ‘ kupitiliza kukhululukilana ndi mtima wonse . ’ Kodi iye anagwilizana nao pa kulambila kwao ? ( Yoh . 7 : 49 ) M’nthawi ya atumwi , Aisiraeli anali kudana kwambili ndi Aroma amene anali kuwalamulila . Misonkhano yathu imatilimbikitsa ndi kutipatsa mphamvu kuti tipitilize kutumikila Yehova ( Mateyu 5 : 41 ) Kodi mungagwilitsile nchito bwanji mfundo imeneyi pa nchito yanu ? Kukambitsilana bwino ndi ana kumathandiza kuwalanga mosasinthasintha . Acinyamata ambili amene afuna kubatizidwa aona kuti mbali imeneyi ndi yothandiza kwambili . ( Miy . 8 : 30 , 31 ) Munthu wodzicepetsa amakhala wokhutila ndi udindo umene ali nawo mumpingo . Kuwonjezela apo , anthu ena ambili - mbili anapwetekedwa maningi . Koma kukamba zoona , sindikuona kugwilizana kulikonse ndi Ufumu wa Mulungu kapena caka ca 1914 . Cifukwa cakuti ena amene poyamba anali kutumikila Yehova , afooka mwauzimu ndi kubwelelanso ku makhalidwe awo akale . Pamene n’nabwelela ku nyumba pa holide mu 1946 , n’napita ku msonkhano wacigawo mumzinda wa Cleveland , ku Ohio , U.S.A . Kodi Baibo ingatithandize kupeza nzelu zothetsela mavuto aconco okhalitsa ndi othetsa nzelu ? Aisiraeli akasonkhana pamodzi na olambila anzawo , anali kupindula kwambili na mayanjano olimbikitsa . Ndakhala ndikutumikila monga mpainiya ku Mongolia kuyambila mu April 2008 . Ndiyeno , Nsanjayo inakamba kuti Satana ayenela kuti sanatenge Yesu ndi kupita naye ku kacisi weniweni mwacindunji . Masiku ano , anthu oposa 240,000,000 amakhala m’dziko lina osati limene anabadwila . Kodi a khamu lalikulu ndi oculuka motani masiku ano ? * Conco , nkhondo ya kumwamba ndi ya padziko lapansi zinacitika m’caka capadela cimeneci . Koma ngati ndi nkhani yaikulu , tingacite bwino kufunsila kwa mkulu kapena kwa m’bale kapena mlongo wofikapo kuti atithandize . Kodi Yehova watilonjeza ciani ? kukhala na nzelu zotithandiza kuti tidzapulumuke . ( b ) Ndi kukambitsilana kwina kuti kumene inu mwapeza kuti n’kothandiza pankhani ya helo ? Mwacitsanzo , ngati mukulimbana ndi maganizo olakwika , musaleme kucita zimenezi . Timaona mosavuta mmene anagwilila nchito yolalikila mwakhama tikamaŵelenga buku la Machitidwe m’Baibulo . Koma pambuyo pake anapatsa Yesu Khristu mphamvu yolamula kuti ukwati uzikhala wa mwamuna mmodzi na mkazi mmodzi , monga mmene zinalili poyamba mu Edeni . — Genesis 2 : 24 ; Mateyu 19 : 3 - 9 . Panthawiyo n’nali na zaka 12 . Cotelo , ubatizo ndi cinthu cofunika kwambili cimene wacinyamata wofikapo mwakuuzimu ndiponso wodzipeleka kwa Yehova angacite . — Miyambo 20 : 7 . Mwa njila imeneyi , n’naphunzila zambili zokhudza Baibo ndi mmene ningaphunzitsile ena zimene imakamba . M’baleyo amawafunsa kuti afotokoze zolinga zauzimu zimene ali nazo . Ana anga James , Jerry , ndi Steven pamodzi na akazi awo akucilikiza nchito yolalikila m’cinenelo camanja m’njila zosiyana - siyana Kuyambila cakumapeto kwa zaka za m’ma 1800 , magazini a Nsanja ya Mlonda anali kufotokoza kuti mizinda yothaŵilako inali na tanthauzo la ulosi . Tingathandize bwanji atumiki anthawi zonse amene akutumikila m’dziko lathu ? 2 : 1 - 3 , 10 ) Ngakhale n’conco , Davide anapempha Yehova kuti apitilize kum’thandiza . — Ŵelengani Salimo 71 : 17 , 18 . Pambuyo pake , Yehova anakana Sauli cifukwa ca kusamvela kwake . Zimene timakamba zingasangalatse ena kapena kuwakhumudwitsa . ( 1 Ates . 2 : 13 ) Dzifunseni kuti , ‘ Nikamalalikila uthenga wabwino , kodi nimayesetsa kupeza mipata yoŵelengela anthu Mau a Mulungu ? ’ Ndipo tikafuna kupanga cosankha , tidzaima na kuganizila mozama mafunso awa : ‘ Ni mfundo za m’Baibo ziti zimene zinganithandize kusankha mwanzelu ? Tingacite bwanji kuti timvetse mmene anthu amene akukumana ndi mavuto akumvelela ? Mizindayo itasankhiwa , inakhala “ yopatulika . ” Mwa kugwilitsila nchito zimene zili pa kamutu kakuti “ Mmene Mulungu Adzakwanilitsila Cifunilo Cake , ” fotokozani . . . 2 : 2 ) Ndi njila zotani zimene akulu aluso amagwilitsila nchito pophunzitsa abale kuti ayenelele kusamalila nkhosa ? Peter wa ku Liberia anali kukonda kunyamula zofalitsa ku sukulu . Ife anthu timabadwa tili kale pa udani ndi Mulungu . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mafunso amenewa . Koma kodi tingakulitse bwanji luso lopanga zosankha mwanzelu ? Tifunika kuŵelenga Mau a Mulungu , kuwasinkha - sinkha , na kuseŵenzetsa zimene taphunzila . Kupitila m’gulu lake la ziŵanda , Satana ali na mphamvu pa maboma onse a anthu . Mwacitsanzo , ena mwa okalamba athu amayesetsa movutikila kupezeka ku misonkhano na kutengako mbali , komanso kulalikila nthawi zonse . M’fanizo lake loyamba , Yesu anakamba kuti colinga cake copitila ku dziko lakutali ndi cakuti “ akalandile ufumu . ” Kodi mungalimbe mtima na kuleka kuceza naye ? Tikakhala pakati pa abale ndi alongo athu auzimu , mavalidwe athu afunika kuonetsa kuti mumpingo muli anthu a makhalidwe abwino . N’ciani cimene mungacite poyembekezela kuti Yehova akuthandizeni ? Kodi mungakonde kudziŵa mayankho azoona pa mafunso anu okhudza Mboni za Yehova ? Masiku anonso , makolo acikhristu amayesetsa kuthandiza ana awo kupanga zosankha mwanzelu . “ Anthu ambili amakonda kukamba kuti , ‘ Uzicita zimene nimakamba , osati zimene nimacita . ’ Ni khalidwe lanji limene ni lofala masiku ano ? Nanga Baibo imakamba ciani za khalidweli ? 20 : 1 - 3 ; 21 : 3 , 4 . Kodi Mau a Mulungu tingawagwilitsile nchito bwanji moyenela mu ulaliki ? Anthu amene anasiyana ndi mpingo akalapa n’kusintha , Mulungu , Atate wathu amene amakhululukila amamulandila ndi mtima wonse . — Yes . Iye anapitiliza kuti : “ Ndimaona kuti ndine wodalitsidwa cifukwa ine ndi mkazi wanga timapitila limodzi mu ulaliki , kuphunzila pamodzi , ndi kulambila pamodzi . Alimiwo anafika mpaka pomupha . Iwo angakhulupilile nkhaniyo ngakhale kuti ndi yacilendo . 6 : 18 , 19 . Mwa kuŵelenga na kusinkha - sinkha mabuku a m’Baibo a Mateyu , Maliko , Luka , na Yohane , tingathe kudziŵa bwino kwambili maganizo a Khristu . Ena angabwele monga otumikila kosoŵa . Inoki anali wa mu m’badwo wa 7 kucokela kwa Adamu . Kodi Satana anaganiza kuti Sara angacitile cinyengo mwamuna wake ndi Yehova ndi kulowa m’cikwati cacigololo ? 43 : 10 - 12 ) Timam’konda Mulungu cifukwa watipatsa mwai wocilikiza ulamulilo wake , ndi kupatsa anthu okhala m’dziko la mavutoli ciyembekezo ceniceni . 4 : 8 , 9 . Kodi mungacite ciani kuti mukhale timu imodzi na mnzanu wa m’cikwati ? Zakeyu , mkulu wa okhometsa msonkho ku Yeriko , analemela kwambili cifukwa colanda anthu ndalama . Kuti cikwati cikhale copambana , aliyense wa aŵiliwo m’banja afunika kucita mbali yake na kumvela Yehova . Nthawi imene inali kundikondweletsa kwambili , ndi pamene tinali kuimba titayatsa moto panja m’madzulo ndi kuseŵela m’thengo ndi anyamata ena . Iwo anafunika kulalikila ‘ uthenga wabwino wa ufumu padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse . ’ — Mat . Mwacitsanzo , m’malo mofunsa mwana wanu mmene tsiku lake layendela , zingakhale bwino kusimba mmene tsiku lanu linalili . Zinalalikila mokhulupilika m’ndende , m’misasa ya cibalo ndi kumadela ena akutali . ( a ) Kuonjezela pa mavuto amene amagwela anthu onse opanda ungwilo , ndi masautso ati amene Akristu amakumana nao ? Kodi n’ciani cinawathandiza kukhalabe okhulupilika ndi omvela ? N’zoonekelatu kuti mkazi ameneyu anafa asanakhale wophunzila wa Yesu ndiponso asanadzozedwe ndi mzimu woyela kapena asanayambe kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu . Zinthu zinasintha mwadzidzidzi . Ni Yehova cabe amene ali na nzelu zimene zingathandize kuti padziko pakhale mtendele . Yehova anamuonjezela zaka zina 15 . Zinthu zina zimene timasankha zimatikhudza ndipo zingakhudzenso anthu ena amene timakonda . 19 : 31 - 37 . ( 1 Tim . 2 : 3 , 4 ) Olo kuti Mulungu amazonda zoipa , amaona anthu kukhala amtengo wapatali kwambili ndipo safuna kuti aliyense akawonongeke . — 2 Pet . Pa tsiku limene n’namasulila nkhani ya M’bale Stewart , iye analengeza ku mpingo wa m’delalo kuti ofesi ya nthambi ifuna abale aŵili kapena mmodzi amene ni apainiya kuti akatumikile pa Beteli . Ŵelengani Mateyu 13 : 47 - 50 . N’cifukwa ciani n’zotheka kukonda Mulungu ndi mtima wathu wonse ? N’ciani cimacititsa mphatso kukhaladi yamtengo wapatali kwa imwe ? Ndipo pamwambo wa Pasika , panali kukhala makapu anai a vinyo . 32 : 4 ) Ponena za Mfumu Yesu Kristu , Yesaya analosela kuti : “ Mfumu idzalamulila mwacilungamo . ” Amenewa ndi abale ndi alongo athu . MMENE YEHOVA AMAONELA ZOFOOKA ZA ANTHU Kuphunzila mmene Yesu anali kucitila ndi anthu kumatipatsa cidalilo cakuti m’dziko latsopano ulosi wa m’Baibulo , wakuti : “ Adzamvela cisoni munthu wonyozeka ndi wosauka , ” udzakwanilitsidwa . 45 : 24 ) Aya ni malangizo amene Yosefe anapatsa abale ake pamene anali kubwelela kwa atate wawo . Yehova analonjeza kuti adzathetsa nkhondo , ndipo siidzakhalaponso . Pamene Davide anapempha Barizilai wa zaka 80 , kuti akakhale ku nyumba ya mfumu , unali mwayi wapadela kwa Barizilai . ( Aroma 1 : 11 , 12 ) Ponena za apainiya a pa mpingo wake , mlongo wina amene anali mpainiya kwa zaka zambili anati : “ Apainiya amalimbikila kugwila nchito mwakhama . Nkhanza zapangitsa akapolo ambili kumenyela ufulu . Lekani ndikufunsenkoni : Mogwilizana ndi zimene Mulungu amafuna , kodi muganiza kuti munthu ayenela kupempha kudzela mwa ndani ? Mu 1952 Pamene n’nali na zaka 17 , nikalibe kungena usilikali Kodi Yehova amatithandiza bwanji kucepetsa nkhawa ? Akatswili ena a mbili yakale amanena kuti anthu oposa 100 miliyoni anafa pa nkhondo m’zaka za m’ma 1900 . Ena anali odzozedwa ndipo anapita kumwamba . Ambili amayamikila zinthu zabwino zimene gulu la Yehova likuticitila . Satana Mdyelekezi amafuna kutilefula cifukwa adziŵa kuti tikalefuka tidzafooka kuuzimu . Iye anacititsa mkazi woyamba , Hava , kusamvela lamulo lakuti asadye zipatso za mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa . ( Gen . 3 : 1 - 5 ; Chiv . Ndiyeno , anzake a ku Canada anam’pempha kuti akalalikile naye ku Mexico kwa mwezi umodzi . Pambuyo potumikila mumpingo wa cinenelo cina kwa zaka zitatu , Serge , na mkazi wake Muriel , anazindikila kuti mwana wawo wa zaka 17 sanali kukondwela na zinthu zauzimu . Akatelo anali kupezelatu mayankho a mafunso ndipo njila imeneyi inathandiza kwambili . Zoonadi , kwa zaka zambili pakhala mibadwo yosiyanasiyana koma Dziko Lapansi lili cikhalile lolimba ndi losagwedezeka pocilikiza zamoyo zosiyanasiyana mpaka pano . Danieli anali mmodzi wa acinyamata amene anasankhidwa kuti atumikile mfumu . Mlongoyu anali kusiya zofalitsa , makalata , ndipo anasiyanso adilesi yake . Coyamba , dziŵa zimene iye amakhulupilila na nkhani zimene angakonde kuti mukambilane . OPEZEKA PA CIKUMBUTSO ( 2016 ) Kuyambila m’nthawi ya atumwi , Satana wakhala akusonkhezela anthu kuzunza kwambili otsatila a Yesu , ndipo zimenezi ndi umboni wakuti iye ndi wankhanza . Iye amandithandizadi kwambili , ndipo n’cifukwa cake ndimamukonda . “ Cenjelani ndi kusilila kwa nsanje kwamtundu uliwonse , cifukwa ngakhale munthu atakhala ndi zoculuka cotani , moyo wake sucokela m’zinthu zimene ali nazo . ” 1 : 9 ) Mukakhala na nkhawa , muzipemphela kwa Yehova ndi kumuuza nkhawa zanu zonse . Popeza kuti unali usiku kwambili , tinaganiza zokambilana nkhaniyo m’maŵa . Kodi n’ciani cimatithandiza kukhala na thanzi labwino ? Iye anatilenganso mwapadela ndipo watilemekeza mwa kutipatsa mtima wofuna kumulambila , ndipo amatithandiza kucita zimenezi . Ehrenbogen ) , Na . Pamenepo kumwamba kunatseguka , ndipo Yohane anaona mzimu wa Mulungu ukutsika ngati nkhunda kudzamutela . Kuwonjezela apo , Mboni za Yehova mamiliyoni ambili pa dziko lonse zakhala abale na alongo anga auzimu . 10 : 1 - 5 . Ndipo muzitsogolela banja lanu pa zinthu zauzimu ndi pa kulambila kwa pabanja . Ngakhale pamene Yosefe anali m’ndende m’dziko lacilendo , Yehova anali kumudalitsa . Conco , aliyense wa ise ayenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi kuimba pa misonkhano nimakuona bwanji ? Iye anati : “ N’zokondweletsa kucita upainiya ku dela kumene anthu ali ndi ludzu la coonadi . Tidzaphunzilanso mmene kuukitsidwa kwa Kristu ku moyo wosafa wakumwamba kumatikhudzila , ndi mmene kumakhudzila nchito yathu monga alengezi a Ufumu . Koma aliyense pamalo pake : Coyamba Kristu , amene ndi cipatso coyambilila , kenako ake a Kristu pa nthawi ya kukhalapo kwake . Na imwe mungakumbukileko atumiki ena okhulupilika akale , amene anadalila Yehova ndi kucitapo kanthu moyenelela . 6 : 8 . Baibulo limati : “ Ngati wina akusoŵa nzelu [ makamaka panthawi ya mayeselo ] , azipempha kwa Mulungu , ndipo adzamupatsa , popeza iye amapeleka moolowa manja kwa onse ndiponso amapeleka mosatonza . ” Pamene tithandiza anthu kuphunzila za Mulungu , timadziŵa kuti Yehovaakusangalala ndi kuti amayamikila khama lathu pa nchito imene watipatsa . Izi n’zosadabwitsa , cifukwa palibe munthu amene anakhalako na moyo umenewu kuti atifotokozele mmene ulili . Kodi lemba la caka ca 2016 ndi liti ? Onani zinthu zotsatilazi . Komanso , iye ndi anzake atatu , Hananiya , Misayeli ndi Azariya , anali odziŵika kwambili cifukwa anasankhidwa mwapadela kuti aphunzitsidwe na kukhala atumiki a mfumu . Ezekieli sanaike cizindikilo anthu amene anafunika kupulumuka . Ndinadziŵa kuti vuto langa lalikulu lidzakhala kupita mu ulaliki . 18 KodI Mukumbukila ? ( Agal . 5 : 16 ) Mwacitsanzo , ganizilani za Nowa na banja lake . Inde . Ganizilani mafunso awa : Kodi mungakhulupilile malonjezo otonthoza a m’Baibulo ngati simudziŵa kuti malonjezowo analimo m’mipukutu yoyambilila ya Baibulo ? Nthawi yacisanu Yesu anaonekela kwa atumwi ake ndi ena amene anali nao pamodzi . 4 : 8 ) Yehova amadziŵa kuti ndife opanda ungwilo ndipo nthawi zambili timakonda kulakalaka zoipa . Boma limenelo ndi Ufumu wa Mulungu umene Yesu anaphunzitsa otsatila ake kuti azipempha kuti ubwele . — Mateyu 6 : 9 , 10 . ( 1 Akor . 10 : 24 ) Mwacitsanzo , pa misonkhano ikulu - ikulu , akalinde amafika mwamsanga ena asanafike . Conco , Yesu anatilangiza kuti : “ Lekani kudela nkhawa . ” Mafanizo onse aŵili ndi cenjezo lakuti Akristu odzozedwa sayenela kukhala oipa ndi aulesi . Mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ’ ” — MAC . 1 : 7 , 8 . Anzanga ena amene n’nali kuwauzako uthenga wa Ufumu naonso akutumikila Yehova tsopano . Iwo amamvetsetsa bwino ngako zinenelo zakale za m’Baibo , ndipo ali na mipukutu imene inapezeka posacedwa . Mwina matenda adzakula ndi kuphonya mwayi wokatumikila ku dziko lina . Ndipo ngati mudalila Yehova , zolinga zanu zidzakwanilitsika . 4 : 9 ) Ngati titsatila malangizo amenewa , tidzapeza cimwemwe cimene cimabwela cifukwa copatsa ena zinthu tili na colinga cabwino . — Mac . 20 : 35 . Iwo amawasamalila monga kuti ndi makolo ao eni - eni . Kodi mwanayo ali ndi zinthu zambili zofunika kusamalila ? Yesu anaticenjeza kuti zimene timayang’ana zingakhudze mtima wathu ndi kudzutsa cilakolako ca kugonana . Ndithudi , Mulungu wapeleka mwai kwa akazi okhulupilika wokwanilitsa mau a wamasalimo akuti : “ Yehova wapeleka lamulo , ndipo akazi amene akulengeza uthenga wabwino ndi khamu lalikulu . ” — Sal . Zinali zovuta kwa amai kupezela zakudya banja lonse . Motelo , tiyenela kuyesetsa kumvela lamulo lake lopewa magazi . Yehova anali kufuna kuti mtundu wa anthu ukhale padziko lapansi kwamuyaya . ( Gen . Mumtima mwanga n’naganiza kuti mwina pano m’pamene Davide anatola miyala isanu yooneka bwino , kuphatikizapo umene anaphela Goliyati . ” ( Mac . 17 : 27 ) Nkhani zotsatila zinai , zidzafotokoza mmene Mulungu amaonetsela cidwi kwa munthu aliyense payekha ndiponso mmene wacitila zimenezi kwa anthu enieni monga inu . [ Mau apansi ] Tikalandila magazini , tinali kukopela mau ake kuti tiziseŵenzetsa pophunzila . ( 1 Atesalonika 2 : 13 ) Mulungu anauzila ophunzila a Yesu Khristu okhulupilika kulemba mabuku amenewa pa nthawi yocepa . Anawalemba pafupi - fupi zaka 60 kuyambila mu 41 C.E . kufika mu 98 C.E . Kodi Satana amaseŵenzetsa bwanji maboma , cipembedzo conama , na magulu a zamalonda posoceletsa anthu ? Abale awo auzimu anawapatsa zakudya na zovala . Ngakhale kuti iye ndi mwamuna wake anali atakumanapo ndi mavuto ambili , aakulu ndi aang’ono , io anali kuona kuti thanzi lao linali cabe bwino . Cinacitika n’ciani Yesu atakhala m’manda masiku atatu ? Iye amagwilitsila nchito mphamvu zake kuti athandize atumiki ake ndi kugonjetsa adani ake . Kukhala paubwenzi wabwino na ena n’kofunika kwambili kuposa cuma coculuka . ( Genesis 40 : 3 - 7 ) Mwina kukoma mtima kwa Yosefe n’kumene kunapangitsa kuti akaidiwo amasuke ndi kumufotokozela mavuto ao . 103 : 10 ) Komabe , monga mmene Davide anauzila Solomo , kuti kulambila kwathu kukhale kovomelezeka pamaso pa Yehova , tifunika ‘ kum’tumikila ndi mtima wathunthu . ’ Ndipo mofanana ndi m’nthawi ya atumwi , timakondwela na cilimbikitso cimeneci . Lemba la Aroma 12 : 2 limati : “ Musamatengele nzelu za nthawi ino , koma sandulikani mwa kusintha maganizo anu , kuti muzindikile cimene cili cifunilo ca Mulungu , cabwino , covomelezeka ndi cangwilo . ” Baibulo limatiuza kuti tifunika kucita zinthu zina zofunika kwambili . N’cinthu canzelu kumvela malamulo a Mulungu olo kuti anthu ena angatiseke . ( Ŵelengani Yakobo 1 : 17 . ) Muzigwilitsila nchito mabuku amene alipo m’cinenelo canu , ndipo ngati n’zotheka , muzisonkhana ndi mpingo wa cinenelo cimene mumamvetsetsa . Gladys Bolton , amene anatumikila mu kafiteliya pa msonkhano wa mu 1937 , anati : “ Ndinakumana ndi anthu ocokela m’madela osiyanasiyana ndi kumva mmene anali kulimbanilana ndi mavuto . Pamene Farao anadziŵa kuti Sara anali mkazi wa Abulahamu , anam’tumiza kwa mwamuna wake , na kuuza banja lonse kuti licoke mu Iguputo . Kodi mungakonde kuŵelenga lembali ? ( Ŵelengani Aroma 12 : 10 . ) Limeneli ndi cenjezo lamphamvu kwa Akristu amene afuna kukwatila kapena kukwatiwa ndi munthu amene sakonda Yehova . Makolo amenewo angakufunseni cifukwa cake simulola anawo kutengako mbali m’zocitika zimenezo . M’kamwa mwake munali kutuluka lupanga lalitali lakuthwa , loti aphele mitundu ya anthu , ndipo adzawakusa ndi ndodo yacitsulo . Conco , anauza mneneli Natani kuti : “ Ine ndikukhala m’nyumba ya mitengo ya mkungudza , koma likasa la pangano la Yehova likukhala m’cihema cansalu . ” Mwacitsanzo , William wa ku Britain atatsitsidwa pa maudindo pambuyo potumikila monga mkulu kwa zaka 30 , anayamba kukwiila akulu ena . Iye anati : “ Ndinaona zonse zimene abale ndi alongo anacita modzipeleka pobweletsa zinthu zosiyanasiyana pambuyo pangoziyo , komanso cilimbikitso cimene anali kupatsa anthu okhudzidwa . Kukhala osiyana ndi anzake kungamuthandizenso kukhala ndi nthawi yambili yocita pulakatisi kuti akwanilitse colinga cake . ‘ Limba Mtima , Ugwile Nchito Mwamphamvu , ’ Sept . Zimene zinacitika pa Pentekosite mu 33 C.E . , zinatsimikizila ciani ? Anthu ena amakaikila ngati Baibulo ni yoona cifukwa ca cipembedzo cao . Masiku ano , ulaliki wa poyela ukucitika m’madela ambili ku Japan , ndipo ofalitsa pafupifupi 220,000 akuwalitsa coonadi m’dziko la Japan . — Za m’nkhokwe yathu ku Japan . Popeza kuti anthu anali kuona balele kukhala cakudya cotsika poyelekezela ndi tiligu , Augustine anafotokoza kuti mikate isanu iyenela kuti inali kuimila mabuku asanu olembedwa ndi Mose ( “ balele ” wotsika anali kuona kuti akuimila “ Cipangano Cakale ” ) Nanga bwanji za nsomba ziŵili ? Mpake kuti iye atamwalila ali na zaka 127 , Abulahamu “ analoŵa muhema kukamulila Sara . ” 147 : 4 ) N’cifukwa ciani iye anayamba kukamba za nyenyezi zakumwamba ? N’cifukwa ciani ndife otsimikiza kuti Yesu amadziŵa bwino cilengedwe ? Pambuyo pakuti cipembedzo conyenga caonongedwa , n’ciani cidzacitikila anthu a Yehova ? Pakati pawo panali munthu wina dzina lake Charles T . Mwacitsanzo , tingapeleke zinthu zocilikizila nchito ya Ufumu pampingo wathu kapena padziko lonse lapansi . Mwacitsanzo , mkazi wawo anali kuzonda Mboni za Yehova . Mwina munamvelapo anthu ena akukamba kuti : ‘ Sin’nali kuyamikila cilango cimene makolo anga anali kunipatsa mpaka pamene n’nakhala ndi ana angaanga . ’ Mneneli wakale Yesaya anafotokoza Mulungu kuti ndi “ amene anaumba dziko lapansi ndi kulipanga , amene analikhazikitsa mwamphamvu , amene sanalilenge popanda colinga , amene analiumba kuti anthu akhalemo . ” Ofalitsa ambili anakondwela ngako na makonzedwe atsopano aulaliki amenewo . Ngakhale kuti panali zopinga zina , iye sanalole zimenezo kumulepheletsa kukwanilitsa colinga cake cokhala mpainiya wa nthawi zonse , ndipo m’kupita kwa nthawi anacikwanilitsadi . Yesu anati : “ Kunena zoona , masikuwo akanapanda kufupikitsidwa , palibe amene akanapulumuka . Koma cifukwa ca osankhidwawo , masikuwo adzafupikitsidwa . ” ( Mat . Tikatelo , mphatso yocokela kwa Mulungu imeneyi idzakhala yodalilika pa umoyo wathu wacikristu . Komabe , pamene anali padziko lapansi anali kukhala ndi anthu opanda ungwilo . 1 : 24 ) Koma , kodi zozizwitsa za Yesu zimatiphunzitsa ciani ? Zotsatilapo n’zakuti Akristu oona aonjezeka . Kodi cikumbumtima cathu cingatithandize bwanji kusangalala ndiponso kupindula ndi zosangulutsa zimene Yehova amavomeleza ? 13 : 6 . Iye “ anatanganidwa ndi nchito zoculuka . ” Kulimbana ndi zofooka zathu : Tingakhale ndi zofooka zimene zimativuta kulimbana nazo kapena tingamalakwitse zinthu zina mobwelezabweleza . ( Ŵelengani Salimo 32 : 8 . ) Koma amayi sanaope . Iwo anasankha kubatizika kuonetsa kudzipeleka kwawo kwa Yehova Mulungu . Kodi n’ndani anapanga maselo amenewa ? NYIMBO : 78 , 139 Otsatila a Yesu a m’nthawi ya atumwi anapewelatu zosangalatsa zoipa . Yehova sanatonthoze cabe Aisiraeli monga mtundu , koma anatonthozanso Mwiisiraeli aliyense payekha . Akanakhala wina , Danieli sembe anakamba kuti , ‘ Masiku 30 cabe osapemphela kwa Mulungu , ni ocepa ! ’ N’cifukwa ciani timaona kuti Yehova amatikonda pamene amatitsogolela ndi kutilangiza ? MUNTHU aliyense amafuna kukhala na umoyo wacimwemwe . Kodi ninganyalanyaze zimene wina wanilakwila kuti nisungitse mtendele ? — Miy . OPEZEKA PA CIKUMBUTSO Tsiku lina pamene ndinali kudwala malungo , ndinalandila kalata kucokela kwa iye kuti ndi wofalitsa wosabatizika , ndipo ndinakondwela kwambili kumva zimenezo . Kuwonjezela apo , Yehova amalemekezeka ngati tim’patsa zinthu zathu zamtengo wapatali . — Miy . Mau a Mulungu amati : “ Danani ndi coipa ndipo muzikonda cabwino . ” Tikacita zimenezi , tidzakhala na mwayi wodzamasulidwa kothelatu ku ukapolo wa ucimo na imfa . ( Machitidwe 20 : 3 - 5 , 22 ; 21 : 29 ) Pamene Terofimo anadwala , Paulo sanamucilitse . Conco , “ ndi dipo lolipilidwa ndi Khristu Yesu , ” Mulungu anatipatsa cosoŵa cathu . — Aroma 3 : 23 , 24 . Ngakhale abululu athu atapanda kuphunzila coonadi , tingakhale na cimwemwe podziŵa kuti Yehova amakondwela pamene timutumikila mokhulupilika . Yehova amakondwela ndi munthu amene amam’tumikila ndi mtima wonse . — Sal . Iye anali wosabeleka , ndipo apa n’kuti wafika zaka 75 . Masako ( Hos . 2 : 23 ) Ulosi umenewu unakwanilitsika pamene Yehova anayamba kusankha anthu a mitundu ina kuti nawonso akhale m’gulu la okalamulila pamodzi na Khristu kumwamba . Mkristu wofikapo akamacita phunzilo laumwini , amafufuza mfundo za m’Baibulo zimene zimam’thandiza kudziŵa cabwino ndi coipa . Mfumuyo inafunikila kwambili thandizo la munthu wina kuti ibwelele pa njila yoyenela . Komabe , amapewa kupangila zosankha abale ndi alongo pa nkhani zaumwini . Ndiyeno , ndinaona matumba a katundu amene sanacotsedwe m’ndekezo . Masomphenya akuyamba motele : “ Ndinaona hachi yoyela . Tiyenela kumvetsela mwachelu pamene akutifotokozela mavuto ao . ( 1 Akor . 5 : 6 , 7 , 11 ) Ndipo popeza Mulungu amapeleka cilango coyenelela , kucotsa munthu mu mpingo kungam’thandize kuzindikila kukula kwa chimo lake na kum’sonkhezela kulapa . — Mac . ( Machitidwe 15 : 29 ) Ngakhale kuti mau othela m’kalatayo anali njila ina yolailila , mauwa amatikumbutsa kuti mwacibadwa anthufe timafuna kukhala ndi thanzi labwino . Kulimba mtima kwa anthu a Ambuye n’kumene kwacititsa kuti tipambane milandu . ” Koma cisangalaloco sicinakhalitse . Tifunikanso kufufuza mayankho a mafunso amene tingakhale nao . Zimenezi zinam’khumudwitsa kwambili , ndipo cinali covuta kwa iye kuwafotokozela kuti waganiza zoyamba kupezeka pamisonkhano . ( Sal . 91 : 14 ) Zoonadi , Yehova Mulungu amatisamalila mwacikondi ndi kutiteteza kwa adani athu kuti asatifafanize . M’mbili yonse , anthu a Yehova akhala akusangalala ndi zinthu zimene ali nazo . N’cifukwa ciani kukhalabe maso n’kofunika kwambili masiku ano ? Timakhudziŵa kwambili tikaganizila zonse zimene Yehova waticitila . Kodi mudzayankha modekha ? Na mapiko awo amphamvu , anafika n’kunyamula ciwiya cimene munali mkazi wochedwa “ Kuipa . ” Tifunika kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova Mulungu . Koma palibe munthu amene anatikondapo kuposa mmene Atate wathu Yehova amatikondela . Kaya akhale ndi zolinga zotani , anthu amene amalemba lembali amakhulupilila kuti cikondi ca Mulungu cidzacititsa kuti akakhale kwamuyaya . Abale amaona ndi kumvetsela mmene umaphunzitsila ena za Yehova . ( Chiv . 20 : 6 ) Iwo anali monga ndodo ya Yuda . Ŵelengani Mateyu 13 : 44 - 46 . Nikhulupilila zimenezi na mtima wanga wonse . 3 : 2 ) Dzikoli , limene wolamulila wake ni Satana , limalimbikitsa anthu kukhala ndi “ cilakolako ca thupi , cilakolako ca maso ndi kudzionetsela ndi zimene munthu ali nazo pa moyo wake . ” ( 1 Yoh . N’cifukwa ciani kufunsa mafunso omvela athu mwauluso n’kofunika ? Tikufalitsa mabuku othandiza kuphunzila Baibulo kwa anthu padziko lonse lapansi Anakamba kuti alimiwo anazunza anthu amene mwini mundayo anawatumiza kwa iwo . Anali bwenzi lao ndipo anali kuona zinthu zabwino mwa io . Komabe , onani zimene Baibulo limakamba ponena za Mulungu woona : 1 , 2 . ( a ) Kodi mau a Yesu a pa Mateyu 24 : 12 anali kukamba za ndani poyamba ? Yehova akutifunsa kuti : ‘ Kodi n’cifukwa ciani iwe ukuopa munthu woti adzafa , ndi mwana wa munthu amene adzakhala ngati udzu wobiliŵila ? ’ — Yes . Komabe , abale athu ena pofuna kutithandiza angatipatse malangizo okhudza thanzi ngakhale kuti sitinawapemphe . 16 , 17 . ( a ) Kodi kubatizika kumakhudza bwanji ciyembekezo cathu ca moyo wosatha ? Luka 3 : 32 imachula anthu enanso asanu pa mzela wa makolo a Mesiya . Kodi Yehova amawadalitsa bwanji anthu ake ? Kodi Baibulo limatithandiza bwanji kuyandikila Mulungu ? Gulu la nkhondo la Aisiraeli linatsika m’philimo ndi kupita kukakumana ndi gulu lankhondo loopsa la adani ao . Nkhaniyo imati , “ mwamsanga [ Rabeka ] anatsika pangamila , ” sanayembekezele ngamila kugwada pansi . Atatelo anafunsa mtumiki kuti : “ Kodi munthu akubwela apoyo kucokela m’chile kudzakumana nafe ndani ? ” Nili kumeneko , n’napita kukaonana ndi a Hardaker kucipatala cawo . Rutherford anapita kukaimilila pa pulatifomu . MWINA munaonapo kuti anthu amene anaona cocitika cinacake , nthaŵi zambili amakumbukila cocitikaco mosiyana - siyana . Yesu anadziŵa kuti paciyeso comaliza , sadzafunika kudalila anthu ena . Koma sangakwanitse kulepheletsa nchito imeneyi . Koma nthawi zina , munthu amene wacita chimo lalikulu angaonetse mzimu wosalapa . Khama limene omasulila zofalitsa zathu ali nalo limandicititsa cidwi . Apa Yesu anaonetsa kuti ndi wodzicepetsa kwambili . Acinyamata amene amatumikila Yehova ndi osiyana kwambili ndi acinyamata a m’dzikoli . Kodi kukumbukila Mlengi wathu Wamkulu kumaphatikizapo ciani ? Ndipo m’mlengalenga mukufotokoza nchito ya manja ake . ” Ndine mlimi , cifukwa munthu wina anandigula kuti ndikhale kapolo wake kuyambila ndili mnyamata . ’ N’ciani cingatithandize tikakumana ndi mavuto aakulu ? N’zosatheka kupewelatu vuto la kusemphana maganizo na acibululu anu osakhulupilila . Tsopano papita zaka zina 39 , ndipo sindinasiye kupemphela . Koma masiku ano popemphela ndimanena kuti , “ Zikomo kwambili Atate wanga wakumwamba cifukwa coyankha mafunso amene ndinali nao pamene ndinali mwana . ” Ganizilani zimene zinacitikila m’bale Willi Diehl . Anandikumbatila ndi kundiuza kuti akumvetsa mmene ndikumvelela , ndipo anandilonjeza kuti adzandithandiza . ” Kuyambila pamenepo , Suntuke anayamba kukayikila Eodiya na kumuganizila zoipa . Baibo imafotokoza momveka bwino colinga ca Mulungu ca poyamba cokhudza dziko lapansi m’mau awa : “ Kunena za kumwamba , kumwamba ndi kwa Yehova , koma dziko lapansi analipeleka kwa ana a anthu . ” ( Salimo 115 : 16 ) Inde , Mulungu analenga dziko lapansi kuti likhale malo okongola , okhalapo anthu kwamuyaya . Nanga n’cifukwa ciani Yosiya anapita kukamenyana naye ? 3 : 11 ) Ngakhale n’conco , Yehova anatidziŵitsa colinga cake cokhudza dziko lapansi ndi anthu . Podzafika mu 1963 , colinga ca M’bale Knorr cinakwanilitsidwa . Anthu amene anapezeka pa Cikumbutso ku Armenia pa April 14 , 2014 anali oculuka kuwilikiza kaŵili poyelekezela ndi ciŵelengelo ca ofalitsa a m’dzikolo Munthu sindiye amacititsa mavuto ambili . Amadela nkhawa kwambili umoyo wa amene akufuna kutumikila Mulungu , ndipo nthawi zambili Yehova wakhala akuwaseŵenzetsa kulimbikitsa na kuteteza atumiki ake okhulupilika padziko lapansi . — Aheberi 1 : 14 . Ndipo sitifuna kuti io ndi anthu oitanidwa akacite manyazi ife tikadzakana kutenga nao mbali m’miyambo yacipembedzo . Cimodzi mwa zinthu zimenezi ndi kucita zinthu zakuuzimu nthawi zonse . Tinganene kuti mwina anasintha zocita zake . “ Dzina lanu ndinu Yehova , Inu nokha ndinu Wam’mwambamwamba , wolamulila dziko lonse lapansi . ” — Salimo 83 : 18 . Komabe , kuti Adamu ndi Hava apitilize ‘ kuyang’anila colengedwa ciliconse cokwaŵa padziko lapansi , ’ anafunikila kukhala ndi moyo kwamuyaya . Iwo anali kudzakondwela ndi nchito imeneyi kwamuyaya . Cimene cinanithandiza ndi malangizo a pa 1 Akorinto 15 : 33 . Pamene Mfumu Davide anali kufotokoza zinthu zofunika pomanga kacisi , iye anavomeleza kuti zonse zimene tili nazo zimacokela kwa Yehova , ndi kuti zonse zimene tingapeleke kwa Yehova n’zocokela kwa iye . — Ŵelengani 1 Mbiri 29 : 11 - 14 . Ndiyeno , Bungwe Lolamulila linatipempha kuti tisakile malo omangapo ofesi ya nthambi yaikulu . Mizela ya makolo a Yesu imene Mateyu na Luka analemba ionetselatu kuti Yesu anali Mesiya wolonjezedwayo . Ngakhale kuti tikalibe kulandila mphoto yathu , tili ndi cikhulupililo colimba cimene cimatithandiza kuyembekezela moleza mtima ‘ mphoto imene tidzalandila . ’ Kutacha m’maŵa , iye anaganizila za kulimba mtima ndi cikhulupililo ca mtsogoleli wao Balaki . Iwo amayamikila ngati ena awatengako pa galimoto kupita nao mu ulaliki , kuwaitana ku cakudya , kuwapatsako kandalama ka mafuta a galimoto kapena kowathandiza kugula zinthu zina . Komabe , atazindikila kuti Kenneth na Filomena ali panja , anatsegula citseko na kuwauza kuti angene . Utumiki umenewu wanithandiza kukhala ndi umoyo wa tanthauzo . ” Ngakhale kuti anthu mamiliyoni ambili amakumbukila imfa ya Yesu , ndi okhawo ali m’panganoli amene ayenela kudya mkate ndi kumwa vinyo . — Ŵelengani Chivumbulutso 5 : 10 . Baseball ni maseŵela a bola amene matimu aŵili amapikisana . Timu iliyonse imakhala ndi anthu 9 . Nayenso Jean - David wocokela ku France analemba kuti : “ Tinalalikila kwa maola ambili mumsewu umodzi cabe . Iye anaonjezelapo kuti : “ Tapindula kwambili kukhala ndi abale amenewa pa mpingo wathu . ” ( 1 Petulo 4 : 8 ) Citsanzo cawo cawonetsa kuti n’zotheka kukhala m’dziko limene mulibe nkhanza . Khalani na Cikhulupililo m’Malonjezo a Yehova , Oct . Betaniya unali mudzi waung’ono umene unali pa mtunda wa makilomita atatu kucokela ku Yerusalemu . 2 : 13 ) Mwacitsanzo , nyuzi ndi mafilimu kapena mapulogalamu a pa TV , zingalimbikitse kukwatilana kwa amuna kapena akazi okhaokha . Ndipo zimenezi zacititsa anthu ambili kuona kuti Baibulo limakhwimitsa zinthu pankhani ya kugonana kwa amuna kapena akazi okhaokha . — 1 Akor . Ndiponso , popeza kuti sanaloŵe m’malo mwa winawake kapena kuloŵedwa m’malo , iye achedwa “ wansembe wamuyaya . ” Ngati tadziŵa kuti tili ndi zizoloŵezi zoipa m’mitima yathu , tingacite bwino kuzicotsa zikalibe kuononga makhalidwe athu . Tsiku lililonse , anthu oposa 1.6 miliyoni amapita pa webusaiti yathu . Nkhondo ili mkati ku Taanaki , mwadzidzidzi kunagwa cimvula coopsa cimene cinapangitsa kuti m’delalo mukhale vimadzi ndi matope okha - okha . Conco , pamene tipitiliza kugwila nchito yolalikila mokhulupilika , timakhala okonzeka kupeleka cilimbikitso kwa anthu panthawi imene akufunikila thandizo . ( Yes . Mofananamo , Yesu , Mkulu wa Ansembe , anapeleka citsanzo cabwino kwa odzozedwa ndi nkhosa zina . Conco , khalani otsimikiza kuti angelo onse amacita cidwi na imwe . Mwina Abulahamu ayenela kuti anakhala pansi coyamba kuganizila mmene angamuuzile . Ndiyeno , anamuuza zimene Yehova anakamba kuti : “ Tuluka m’dziko lako ndi pakati pa abale ako . Tiye ukaloŵe m’dziko limene ine ndidzakusonyeza . ” N’cifukwa ciani Msulami anakonda m’busa ? Akuluakulu a boma akayesa kukuletsani kulambila Mulungu , zingaoneke ngati kuti moyo ndi tsogolo lanu zili m’dzanja mwao . Mosayembekezela , tinalandila kalata yocokela ku ofesi ya nthambi yotipempha kuti tiyambe kutumikila monga apainiya apadela akanthawi . Iye anali kucitila cithunzi mfumu yosatha komanso wansembe wamtsogolo . Kodi mngelo anamulimbikitsa bwanji Danieli ? Mwacitsanzo , kuonjezela pa ulaliki wa khomo ndi khomo , tingacite ulaliki wa m’makalata , wa pafoni , wa mu mseu ndi kumalo ena kumene kumapezeka anthu ambili , ndiponso kulalikila anthu mwamwai ndi ku malo a malonda . Dipo lidzabweletsela anthu moyo wamuyaya . Koma kuti akapeze moyo umenewo , afunika kucitapo kanthu . Kholo lililonse lingam’kwiile munthu woipayo . A Zimba : Ndi mmenemo . Yehova anali kuyembekezela kuti Mfumu Zedekiya adzacita zinthu mogwilizana na lumbilo limene anacita m’dzina la Mulungu . Yelekezani kuti mukumuona akudziwongola manja . Ngati tifuna kuyandikila Yehova , tiyenela kuyesetsa kupitiliza kutengela iye ndi Mwana wake Kucokela paciyambi , Yehova anali kufuna kuti padziko lapansi padzaze ana angwilo a Adamu na Hava . ( Gen . ( 3 ) Kodi tingatengele bwanji Yehova na Mwana wake pamene tipatsa ena cilango ca uphungu ? Conco , mu 1961 atatipempha kuti tikatumikile monga apainiya apadela ku Falls City , m’dela la Nebraska , tinavomela . Zinatheka cifukwa cakuti olembawo anauzilidwa ndi Mulungu . — Ŵelengani 2 Samueli 23 : 2 . ( Sal . 37 : 4 ) Ngati tiika zinthu za kuuzimu pa malo oyamba m’moyo wathu , ndiye kuti tikukonzekela kudzakhala ndi moyo weniweni mtsogolo . — Ŵelengani Mateyu 6 : 19 - 21 . Mlongoyu anali kuthandiza mlongo wina wamasiye dzina lake Carol . Malinga ndi mwambo , io anacita pangano la ukwati pakati pa Rabeka ndi Isaki . N’cifukwa ciani Yesu anali kugwilitsila nchito mafanizo ? Mabwenzi ake apamtima anali atumwi ndipo io anali okhulupilika ndi omvela kwa iye . Pofika nthawi ya Nowa , dziko lapansi “ linadzaza ndi ciwawa . ” ( Gen . Iye anasoketsela mwana wake ameneyo covala cabwino kwambili . Ena akayamba kugwilitsila nchito Intaneti , angaganize kuti uthenga umene ulipo ndi woona cifukwa cakuti uli pa Intaneti , kapena cifukwa cakuti mnzao wawatumila pa imelo . N’ciani cimene tiyenela kukumbukila tikamalalikila anthu othaŵa kwawo ? Umenewu ni umboni wakuti Ufumu wa Mulungu ukulamulila , ndipo posacedwa udzabweletsa madalitso osaneneka pa dzikoli . Ndiye cifukwa cake anthu anali kukhala na moyo zaka zambili . Kudziŵa mayankho a mafunso amenewa kudzatithandiza kupilila . Lembali limati : “ Kugwilizana ndi anthu oipa kumawononga makhalidwe abwino . ” Iye anati : “ Yemwe anene uthenga wokhudza moyo wa inu Farao ndi Mulungu osati ine . ” — Genesis 41 : 14 - 16 . Kucita zimenezi kukanawathandiza kupitiliza ‘ kubala zipatso m’nchito iliyonse yabwino , ’ makamaka panchito yolalikila uthenga wabwino . 17 : 27 , 28 ) Watipatsanso mphatso yamtengo wapatali — Buku lake , Baibo . Wamasalimo anadziŵa kuti Mulungu anali kuwakonda anthu ake a m’nthawi yakale . 27 Mmene Gayo Anathandizila Abale Ake Baibo siifotokoza zambili pankhaniyi . 37 : 11 Mwacitsanzo , m’bale wina dzina lake Daniel anacita chimo lalikulu , koma kwa miyezi yambili anali kuopa kuulula chimolo kwa akulu . Kwa kanthawi ndithu , mtumwi Petulo anali kucitila tsankho anthu amene sanali Ayuda . Koma m’kupita kwa nthawi anacotselatu tsankholo mumtima mwake . ( Mac . 10 : 28 , 34 , 35 ; Agal . Kukhala wolimbikila nchito n’kopindulitsa m’njila zambili cifukwa cakuti anthu ambili m’dzikoli ni osalimbika pa nchito . — Mlaliki 3 : 13 . Ndipo tiphunzilapo ciani za ufulu wa ena ? Tiyeni tione citsanzo ca m’Baibo coonetsa kufunika kolemekeza ufulu wa abale pa nkhani zokhudza cikumbumtima . Nanga Yehova kupitila mwa Yesu anawakonzekeletsa bwanji kuti awakwanilitse ? Iye anali akali ndi mphamvu . Atayamba kumila , Petulo anafuula ndi kupempha Yesu kuti am’thandize . Tumikilani Yehova mosangalala mukali acinyamata . Nchito yawo inali kulonda mzinda , ndipo akaona kuti adani akubwela , anali kucenjeza anthu mu mzindawo . Iye anasunga ndalama ndi kugulitsa zinthu zina zimene anali nazo . Pambuyo pake anasamukila ku Russia mu 1992 . ( Yesaya 26 : 9 ) N’zoonekelatu kuti padzakhala zinthu zoculuka zimene tidzaphunzila ndi kuphunzitsa ena motsogoleledwa ndi Mfumu yathu , Yesu Kristu . ( Mateyu 6 : 11 ) Pamene tiyamikila cakudya cokoma , sitiyenela kuiŵala kuti Yesu ndi “ mkate wamoyo . ” Otsatila a Yesu anaphunzila kuti cikhulupililo n’cofunika pokhululukila ena . 84 : 7 ; 1 Pet . Phula lopezeka m’cilengedwe lili mitundu iŵili , lamadzimadzi ndi louma . Ndiyeno tsegulani lemba la 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 . Mnzakeyo ataona kuti Chris akuyesetsa kusintha khalidwe lake , nayenso anayamba kusintha . Zonsezi zimaonetsa kuti mau ouzilidwa a Mfumu Solomo ni oona . Iye anati : “ Munthu wapweteka munthu mnzake pomulamulila . ” — Mlal . Tikuyembekezela mwacidwi nthawi yabwino imeneyo . Tiyenela kuphunzila ndi kumvetsetsa mfundo zimene panazikidwa Cilamulo . “ Mkazi wamkulu wa mfumu ” akusangalala pamodzi ndi mkwatiyu . Koma bwanji ngati mwadziŵa kuti Baibo ingakuthandizeni kukhala na umoyo wabwino ndi wacimwemwe ? Mau a pa Malaki 3 : 1 - 3 amafotokoza zocitika za pakati pa 1914 mpaka kuciyambi - yambi kwa 1919 , pamene “ ana a Levi ” odzozedwa anali kudzayengedwa . Koma Yesu anawalonjezanso kuti ‘ Atate adzalemekeza ’ otsatila ake ndi kuwapatsa moyo wosatha . Kodi Yehova amapeleka bwanji citonthozo ? Kodi mtumwi Paulo anawalimbikitsa bwanji Akhristu oyambilila ? ( Sal . 94 : 20 ) Pokambilana na M’bale J . Kodi Angelo Aliko Zoona ? 3 : 12 ) Adolfo , woyang’anila dela wa ku Spain , akumbukila bwino mmene umoyo wake unalili asanaphunzile coonadi . ( 2 Sam . 13 : 1 , 2 , 10 - 15 , 28 - 32 ) Makolo angathandize ana awo kucita zinthu mwanzelu ndi kukhala odziletsa pa nkhani ya cikondi ca pakati pa mwamuna ndi mkazi . Angacite zimenezi mwa kukambilana nawo pa kulambila kwa pabanja nkhani za m’Baibo zimene tachulazi . “ N’liti Pamene Tidzakhala na Msonkhano Wina Waukulu ? ” Masiku anonso , n’zolimbikitsa kuona kuti abale ndi alongo m’mipingo ndi ogwilizana mosasamala kanthu za kusiyana kwa mautumiki kapena udindo . Ifenso tili ndi mwayi umenewo . — Malaki 3 : 6 ; Yakobo 1 : 17 . Koma zoona zake n’zakuti kukhala na ufulu wopanda malile kumabweletsa mavuto . N’zoona kuti ufulu uli na ubwino wake . Mungafunse ku ofesi ya nthambi m’dziko lanu kuti mudziŵe mmene mungacitile zimenezi . Posacedwapa maofesi a nthambi angapo anawaphatikiza pamodzi . ( b ) Nanga n’ciani cimene timadziŵa ponena za Ufumu wa Mulungu ? Naonanso kuti m’bale ni m’bale ndithu , kaya akhale wakuda kapena mzungu , ndipo angathe kukufela pakakhala pofunikila . Kucokela pa zimene zinawacitikilazi , anthu a ku Simeulue akaona zimene zikucitika pa nyanja , amadziŵa kuti kubwela tsunami . Hachi yoyela , imene wokwelapo wake ndi mfumu ya kumwamba . Koma kodi io angathe kugwila nchito imene Mboni za Yehova zikugwila masiku otsiliza ano ? Njila imeneyi yaonetsedwa m’bokosi yakuti “ Phunzilani za Anthu Ochulidwa m’Baibo Kuti Muimvetsetse . ” ( Sal . 145 : 16 ) Potsanzila Atate ake , ‘ Kristu , mphamvu ya Mulungu , ’ nthawi zambili anali kutambasula dzanja lake ndi kukhutilitsa zokhumba za otsatila ake . Ndisanabatizike ndinapempha alongo aŵili aja kuti ndipite nao mu ulaliki wa kunyumba ndi nyumba , kuti ndidziŵe mmene nchito yolalikila imacitikila . ( Mac . Yehova amaona zimene timacita mseli ndipo amationgolela tisanaononge ubwenzi wathu ndi iye . Mofanana ndi Yesu , tiyenela kusankha nthawi yabwino yokamba zinthu , kusankha bwino zokamba , ndi kuyesetsa kukamba mokoma mtima nthawi zonse . Mwacitsanzo , Salimo 135 imakamba za olambila Yehova okhulupilika a m’nthawi ya Isiraeli kuti anali “ cuma cake capadela . ” ( Sal . ( 1 Sam . 10 : 27 ) Mfumu Sauli analola mzimu wa Mulungu kuti umutsogolele ndi kuthandiza Aisiraeli kugonjetsa Aamoni . Tsopano Julio atumikilanso monga mkulu . Iye anati : “ Sindikudandaula kuti ndinayembekezela kwa zaka zambili . ” ( 1 Yoh . 4 : 8 ) Mwa kugwilitsila nchito cinyengo , Satana amalepheletsa anthu ‘ kuzindikila zosowa zao zauzimu . ’ ( 1 ) Eliya atauza Mfumu Ahabu kuti Yehova adzabweletsa cilala , iye anakamba motsimikiza kuti : “ Pali Yehova Mulungu wamoyo , Mulungu wa Isiraeli amene ndimam’tumikila , sikugwa mame kapena mvula . ” 18 , 19 . ( a ) Kodi tiyenela kucita ciani tikayamba kutalikilana ndi Mulungu ? Izi n’zimene anzake anafunika kucita . — Maliko 14 : 32 - 41 . Satana amadziŵa kuti ndi cibadwa cathu kufuna kucita zinthu zoipa , ndipo amafuna kuti tizicita zimenezo . A Daka : Cabwino tidzakambilana . Zioneka kuti pa anthu 1 biliyoni amene amakoka kwambili fodya , ambili adzapitilizabe kufa . • Kodi Mulungu ndi amene amacititsa zinthu zimenezi ? Nanga ndani afunika kuona nchito yanu ? “ Ubwenzi wolimba ndi Yehova ndi wa anthu amene amamuopa . ” — SALIMO 25 : 14 . Cinanso , ngati munthu wapsa mtima , saganiza molongosoka . Ndani amene tiyenela kumukonda koposa ? Nanga n’cifukwa ciani ? Baibulo limaonetsa kuti Yehova amakhumudwa kwambili ngati tiganizila zinthu zoipa kapena kuzicita . Cikhulupililo ni mphamvu imene imasonkhezela munthu kucita zinthu zogwilizana na cifunilo ca Mulungu . DZIKO : ITALY Miseu ya kudela kumene tikhala ili ndi micenga , ndipo ndi yovuta kuyendamo . Nthawi ya mvula imakhala ndi matope . Popatsana moni tinali kunena kuti “ Okonzeka Nthawi Zonse . ” Atumiki ena a Mulungu zimawavuta kulankhula zimene zili mumtima mwao . “ Yehova ali pafupi ndi anthu a mtima wosweka . Ndipo odzimvela cisoni mumtima mwawo amawapulumutsa . ” — Sal . Mungapeze malangizo ena othandiza pa nkhani ya kukhala na zolinga zauzimu m’nkhani yakuti “ Khalani ndi Zolinga Zauzimu Kuti Mulemekeze Nazo Mlengi Wanu , ” yopezeka mu Nsanja ya Olonda ya July 15 , 2004 . Izi zimatipatsa umboni wina wakuti zinthu zakale zofukulidwa m’mabwinja zimaonetsa kuti Baibo n’lolondola ponena za mbili yakale . Ngati mufuna kudziŵa bwino anthu ochulidwa m’Baibo , mungayese kuiphunzila motsatila maina a anthu a m’Baibo . Kuwonjezela apo , zimene Yesu Khiristu anakamba zokhudza Davide zionetsa kuti Davideyo anali munthu weni - weni . ( October 1 , 2012 ) ; “ Kodi Mulungu Amamva Cisoni Tikamavutika ? ” Kodi anacitapo ciani ? Koma kodi ni anthu ati amene Mulungu amawayanja na kuwadalitsa ? 27 ‘ Abale Okhala Ngati Amenewa Muziwalemekeza Kwambili ’ YANKHO : Yehova , Atate wa Yesu , ni Mulungu wosatha , Wamphamvuyonse , ndipo ni Mlengi wa zinthu zonse . Kodi iye sanali kudziŵa kuti ngati sadzamvela Yehova adzafa ? Komabe , iye anali kupewa kukhala nao pacibwenzi . “ Anthu okonda kucita zoipa sangamvetse cilungamo , koma amene akufunafuna Yehova amamvetsa ciliconse . ” — MIY . Munthu wakale amene analembako Baibulo , anaona kuti moyo ndi waufupi kuyelekezela ndi mfundo yakuti dziko lapansi linalengedwa kuti likhale kosatha . Ku Paris , m’nthawi ya Langton , ophunzila a m’maiko osiyanasiyana anabwela ndi Mabaibulo ao . Nthawi zina , khungu la Daniel linali kuoneka buluu cifukwa cosoŵa oxygen m’thupi . Oxygen yambili inali kucoka m’thupi lake cifukwa ca mibowo iŵili imene inali mkati mwa mtima wake . Kodi simuona kuti anthu sayamikila ndipo sakumva za ena ? Conco anayamba kuuza asilikali molimba mtima kuti angathe kugonjetsa Goliyati . Koma tinali okondwela polengeza mau a Yehova pa zisumbu zimenezi . — Yer . Inde , ndi Satana yemweyo . Anthu ambili amaona kuti kuŵelenga Baibo n’kolemetsa . Panthawi yoyenela . Ngati muli ndi mwai woŵelenga nkhani zakuti “ Kodi Baibulo Limaphunzitsa Ciani ? ” Nafenso , cikhulupililo cathu cingatithandize kucita zinthu zimene zingaoneke ngati zosatheka . Kodi tikambilana mafunso ati okhudza cikhulupililo ca Mose coona “ Wosaonekayo ” ? Anthu amenewa ni Mboni za Yehova . Koma anali kucilitsa ziwalo zoonongekazo . ( c ) Kodi Yesu anasonyeza ciani mwa kukhala wokhulupilika mpaka imfa ? Yobu anauza anzakewo kuti cikanakhala kuti iwo ni amene anali kuvutika , ‘ akanawalimbikitsa ndi mau a m’kamwa mwake , ndipo citonthozo ca milomo yake ’ cikanawatsitsimula . Tisamangotsutsa ziphunzitso zilizonse zabodza zimene amakhulupilila . ( 2 Akorinto 9 : 15 ) ‘ Mphatso yaulele ’ yocokela kwa Yehova ndi zinthu zonse zimene iye amatipatsa kudzela mwa Yesu Kristu . Ndipo , Baibulo limalonjeza kuti kudzakhala “ kuuka kwa olungama ndi osalungama omwe . ” Tikamacita zinthu zimene Mulungu amatiuza , iye amatithandiza . Katswili wina wofufuza zimene nkhani za m’Baibulo zimaimila anakamba kuti zimene Yakobo anacita pogula ukulu wa Esau ndi cakudya cofiila , zinaimila coloŵa ca kumwamba cimene Yesu anagulila anthu pogwilitsila nchito magazi ake ofiila . ( Yoh . 18 : 36 ) Yesu sanafune kutenga mbali m’zandale cifukwa Ufumu wake ni wakumwamba . M’malo mwake abale akewo anamucita zacipongwe . 28 : 20 ) Iye anali kudziŵa bwino mmene mzimu woyela , angelo , ndi Mau a Mulungu anam’thandizila kutsogolela anthu pamene anali padziko lapansi . N’ciani cingakuthandizeni kucita zimenezi ? * Panopa , malemba ambili ali ndi mau ocepa kuposa kale , koma matanthauzo ake sanasinthe , ndipo ndi osavuta kumvetsa . Koma ine ndikukuuzani kuti aliyense woyang’anitsitsa mkazi mpaka kumulakalaka , wacita naye kale cigololo mumtima mwake . ” Kuti tiphunzile mmene tingacitile zimenezi , tiyeni tikambilane zocitika zingapo zimene zimafuna kupanga zosankha mwanzelu . N’citsanzo cabwino cotani nanga kwa akulu , pamene aphunzitsa ena kutenga maudindo aakulu mu mpingo . Mosakaikila , mumatha kufika ena pamtima powaphunzitsa coonadi ca m’Baibo . Iye anayamba kukoka fodya ali wacinyamata . Aja amene adzaukitsidwa padziko lapansi , adzakhala ndi ciyembekezo ca moyo wosatha , osati moyo wosafa . Kodi Yehova amayankha bwanji pempho lathu lakuti musatiloŵetse m’mayeselo ? ( Luka 2 : 8 - 14 ) Kenako , abusawo anapita kukaona mwanayo . ( Salimo 49 : 8 ; 1 Petulo 1 : 18 , 19 ) Nanga n’cifukwa ciani Mulungu anapeleka moyo wa Mwana wake monga mphatso ya anthu onse ? Pamene pangano la Cilamulo linali kugwila nchito , ansembe anaikidwa kuti azitumikila mu Isiraeli . Tingawayamikile mocokela pansi pamtima pa makhalidwe abwino ndi maluso amene ali nao . Kodi fanizo limeneli likutiphunzitsa ciani ? Iyai , cifukwa gulu la nkhosa limakhala pamodzi ndipo limatsatila m’busa . Masiku ano , odzozedwa amene ali m’gulu laciŵili la “ m’badwo uwu ” ndi okalamba . Koma iwo anali kucotsa anthu kwa Yesu , “ Mtumiki Wamkulu wa moyo , ” na kuwatsogolela m’njila yopita ku ciwonongeko camuyaya . ( Mac . Anthu ena ocilikiza cipani anazindikila kuti tinali a Mboni za Yehova , ndipo anatiuza kuti tikhale pakati pa gulu landale la acinyamata ( Malawi Young Pioneers ) . Tingaonetse bwanji kuti timawaganizila abale ocokela ku maiko ena kapena abale osauka amene ali mumpingo mwathu ? Kodi mumakonda kumvetsela nkhani , maseŵelo , zitsanzo , ndi mbali zofunsa mafunso pamisonkhano imeneyi ? Panthawi imodzi - modzi , tiona kuti pafunikabe anchito ambili . Ndipo ngakhale kuti mneneli Mikaya anamucenjeza , iye anapitabe ndi Ahabu kukamenyana ndi Asiriya . Tingatengele cikhulupililo ca Sara mwa kuika zinthu zauzimu patsogolo m’malo mwa zakuthupi , kuuzako ena za Mulungu , na kucilikiza mokhulupilika mfundo zake za makhalidwe abwino tikakumana ndi mayeselo . Kupilila Ziyeso Kumabweletsa Madalitso ( P . 9 / 15 ( Danieli 2 : 44 ) Iwo amatsatila citsanzo ca Yesu mwakuonetsa “ kuwala ” kwao ndipo zimenezi zimaonekela pamene acitila anansi ao zinthu zabwino . Nanga iyenela kutilimbikitsa kucita ciani pamene tikukonzekela Cikumbutso ca imfa ya Kristu cimene cidzacitika pa Citatu , pa March 23 , 2016 ? Iwo amakondana kwambili ndipo amasonyezana cikondi . Cifukwa kucita zimenezo kunali ngati kulumphila m’dziŵe lozama kwambili kwa nthawi yoyamba . ” Koma nikali kulimbana ndi mtima wa tsankho , ndipo nthawi zina zimanivuta kupewa khalidweli . Ndi njila ziti zimene ayenela kuseŵenzetsa ? Iwo analandila uphungu wa mkuluyo na kuuseŵenzetsa . Mulungu walonjeza boma la padziko lonse limene lidzathetsa mavuto onse . — Ŵelengani Daniel 2 : 44 . Ndani anali kudzamvetsetsa uthenga wa Mulungu ? Ngakhale n’conco , mkazi wacikhristu amacita zimene angathe kuti aphunzitse ana coonadi . ( Mac . Komanso , acicepele ambili amapita patsogolo ngati akhala na anzawo okhwima mwauzimu , amene angamapite nawo mu ulaliki kapena kucita nawo zosangulutsa zina zoyenela . ( Miy . Kodi ine ningakwanitse kucitako utumiki umenewu ? ’ Kusintha kwa zinthu pa umoyo wa Rabeka kunayamba ndi zinthu zimene anazoloŵela kucita . Tikamayesetsa kulandila cilango ca Yehova ndi kusintha kuti tim’kondweletse , timaonetsa kuti timayamikila citsogozo cake ndiponso kuti timam’kondadi . — Yohane 14 : 31 ; Aroma 6 : 17 . Timaona kuti ndi mwai waukulu kuthandiza abale a Kristu kulalikila . Timawathandizanso mwa kupeleka ndalama ndi kucita khama pomanga Nyumba za Ufumu , Nyumba za Misonkhano , komanso maofesi a nthambi . Kuyankha mafunso amenewa kunafunika nthawi kuti zolengedwa zonse za nzelu zizindikile kuti ulamulilo wa Yehova ndi wabwino kwambili . Nkhani yotsatila idzafotokoza mfundo zimene zingakuthandizeni . Sitikudziŵa amene adzatsogolela mitundu ya anthu poukila anthu a Mulungu , koma ndife otsimikiza kuti ( 1 ) Gogi wa Magogi ndi asilikali ake adzagonjetsedwa ndi kuonongedwa , ndipo ( 2 ) Mfumu yathu , Yesu Kristu , idzapulumutsa anthu a Mulungu ndi kuwaloŵetsa m’dziko latsopano mmene mudzakhala mtendele ndi citetezo ceniceni . — Chiv . A Russell atamwalila , Jordan anauzidwa kuti a Russell anali kuthandiza kwambili ambuye ake aamuna ndi makolo ake . Iwo anali kuwalimbikitsa panthawi ya mavuto . ( Onani palagilafu 13 ) Kodi Yehova amapeleka bwanji njila yopulumukila kwa anthu amene amam’dalila panthawi ya mayeselo ? M’nkhani yaciŵili , tidzaona mmene Malemba amaunikila bwino udindo wa mwamuna ndi wa mkazi m’banja . N’zoona kuti akanatha kupemphela cam’seli kuti ena asamuone . Kodi timangoŵelenga nkhaniyo mwa patalipatali kapena kupewelatu kuiŵelenga ? 11 : 15 . Iwo anali kubwela kucokela “ pamaso pa Ambuye wa dziko lonse lapansi , ” ndipo anatumiwa kukacita nchito yapadela . Motelo , onetsetsani kuti kutumikila Yehova ndiye cinthu cofunika kwambili kwa inu . — Ŵelengani Afilipi 1 : 10 . Nanga bwanji za mnyamata wamanyazi uja ? Kodi kudzicepetsa kumaphatikizapo ciani ? Ngakhale atumiki a Yehova akale , monga Mfumu Davide , anakumana ndi “ masautso . ” ( Sal . Mwacitsanzo , tikaona kuti olambila anzathu alibe zinthu zina zofunika , tingagaŵane nao zinthu zimene ife tili nazo . M’nthawi imene Paulo anali kulemba kalata yopita kwa Aefeso , lupanga limene asilikali aciroma anali kuseŵenzetsa linali lalitali masentimita 50 . Pamene ophunzila Baibulo anali kuculuka , ciŵelengelo ca malo komanso anthu ofika pa Cikumbutso cinali kukwelanso . Ine , amayi , na Grigory , tinali kulalikila m’midzi ya pafupi ndi mzinda wa Tulun , koma tinali kucita izi mosamala . Kodi mumasinkhasinkha mmene mungathandizile ophunzila Baibulo ? Kumbukilani kuti kudzikuza kwa Hezekiya kunaonekela bwino pamene Yehova anagonjetsa Senakeribu , ndi kucilitsa Hezekiyayo pamene anadwala matenda aakulu . Pambuyo polandila malangizo , iwo anapita kukalalikila . Aheberi 5 : 14 ) Mtumwi Paulo anati : “ Aliyense ayenela kunyamula katundu wake . ” — Agalatiya 6 : 5 . KWA MAKOLO Ndipo Ayuda okhala mumzindawo anali kucita kutuluka pacipata ca mzinda n’kukasonkhana m’mbali mwa mtsinje kuti alambile Mulungu . ( Mac . Ndiponso , Yehova amayankha mapemphelo athu kupyolela m’Baibulo . Timafika pomvela monga mmene wamasalimo wina anamvelela . Cinthu cacinai cimene cingatithandize kuti tisatenge mbali m’ndale ndi kuganizila zitsanzo za atumiki a Yehova okhulupilika . Anthu a Yehova ali ngati mtundu waukulu . 4 : 25 . Conco , anawafotokozela colinga ceni - ceni ca utumiki wake . Kayla , mtsikana wazaka 19 anati : “ Ndimakambilana ndi atate nkhani iliyonse . ( Agal . 6 : 7 ) Koma tiyenela kukhulupilila kuti ngati tinalapa , Yehova adzaticilikiza m’mavuto athu , olo kuti mavutowo ni odzibweletsela tekha . — Ŵelengani Yesaya 1 : 18 , 19 ; Machitidwe 3 : 19 . BAIBO IMAYANKHANSO MAFUNSO OFUNIKA KWAMBILI MU UMOYO , MONGA AKUTI : Mwacitsanzo , Baibo imalangiza mkazi kuti “ azilemekeza kwambili ” mwamuna wake . ( Aef . ( Genesis 1 : 31 ) Koma ucimo unaloŵa m’dziko kudzela mwa munthu woyamba , Adamu . Inoki anagona mu imfa ali na umboni umenewu wakuti Yehova akukondwela naye . N’cifukwa ciani anthu okonda ndalama sakhala na cimwemwe ceni - ceni ? Mwacitsanzo , iwo amalimbikitsa mfundo yakuti cuma na ndalama zambili ndiye zimapatsa munthu cimwemwe ceni - ceni . ( Miy . SADZABWELA NDI ZOCITA ZA ANTHU KAPENA ZINTHU ZAKUGWA KUTHAMBO . N’naukila ku cipatala , apo n’kuti nilibe manja . Iwo amamvetsa cisoni kwambili ngati anthu amene Yehova anawauza kuti : “ N’cifukwa ciani anthu inu mukuwononga ndalama polipilila zinthu zimene si cakudya , ndipo n’cifukwa ciyani mukuvutika kugwilila nchito zinthu zimene sizikhutitsa ? Mwakutelo dziko lingapitilize kucilikiza moyo kwamuyaya . Tsiku lotsatila Samueli ataona Sauli , Yehova anauza mneneliyo kuti : “ Ameneyu ndiye munthu ndimakuuza uja . ” Ni makhalidwe ati a anthu a Mulungu amene amaonekela ngako pakagwa masoka ? Zimenezi ziphatikizapo ulosi wonena za lonjezo lakuti “ mbeu ” yapadela idzathetsa nkhani ya ulamulilo wa cilengedwe conse . Tsiku lina , banjali linacita cidwi pamene munthu wina anaima pa kasitandi kawo ka ulaliki na kuwapatsa maluwa okongola . Komanso munthuyo anawayamikila kaamba ka nchito imene amagwila . Ndiyeno masisitele anaganiza zondilekanitsa ndi abale anga . Tiyeni tikambilane za anthu aŵili amene anacita zimenezi . Malonjezo a Mulungu ni odalilika kwambili . Mulungu amafuna kuti tikapulumuke ndipo amatiuza zofunika kucita . Pa cifukwa cimeneci , Yesu anakamba kuti : “ Onani Mwisiraeli ndithu , amene mwa iye mulibe cinyengo . ” Nthawi zina , mungawagaŵe na wacicepele kuti aziwathandizako pamene ayenda m’gawo . Adani ake anali kumupitikitsa ali wokwiya kwambili cifukwa ca uthenga wake wa ciweluzo . Eduardo anati : “ Kucita zimenezi ndi mbali ya cikhalidwe cathu . Koma pali malile ocitila zimenezi . Ndipo timalalikila uthenga wabwino ndi cikhulupililo ndi cidalilo cifukwa uthenga wathu umacokela m’Mau a Mulungu , Baibulo . Malonjezo a m’Mau a Mulungu adzakwanilitsidwa ndithu . Pasanapite nthawi , Riana anakhala na colinga cokatumikila kosoŵa . “ Uyenela kudziŵa bwino maonekedwe a ziŵeto zako . ” — MIY . Kucita zimenezo kumabweletsa mavuto . Kodi nimayesetsa kuthandiza ena , kaya a mu mpingo kapena amene nimapeza mu ulaliki ? ’ 2 : 14 ) Akristu ambili agwela m’chimo cifukwa coyamba khalidwe loipa mwa kupenyelela zamalisece , kuŵelenga mabuku odzutsa cilakolako ca kugonana , kapena kuonelela zinthu zonyansa pa Intaneti . Patapita nthawi , anabwela na anzake ena owonjezeleka . Ngati tisoŵa njila yopezela zinthu zimenezi , mwacibadwa timada nkhawa , ndipo ngakhale Yesu anali kudziŵa zimenezi . Koma sikuti ndalama ndiye vuto . Pamene tipanga maulendo obwelelako ndi kutsogoza maphunzilo a Baibulo , timakhala okondwa kuti timathandiza anthu kutsatila miyezo yolungama ya Mulungu . Nanga anakwanitsa bwanji kukuka ? — Luka 14 : 28 . Patapita nthawi , M’bale Klein analemba kuti : “ Ngati tisungila m’bale wathu cakukhosi , makamaka ngati m’baleyo ndi woyenelela kutipatsa uphungu , tingagwele mumsampha wa Mdyelekezi mosavuta . ” Ngati ena anali kudziŵa , sanatiuze . ” — Edith Brenisen . Mboni za Yehova zimalalikila coonadi m’Cisipanishi ndi m’Ciguarani . Izi ndi zinenelo zimene zimakambidwa ndi anthu ambili m’dzikoli ( Miyambo 6 : 20 ) Mungagwilitsile nchito malangizo a pa jw.org othandiza pophunzitsa kuti muthandize ana anu kuganizila mwakuya nkhani imene akuphunzila m’buku la Baibo Imaphunzitsa ndi kudziŵa mmene angagwilitsile nchito zimene akuphunzila . — Pitani pa ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA . Mwacitsanzo , zikhoza kuononga mbili yabwino ya munthu , kapena ya gulu linalake . Mungaseŵenzetse bwanji Mateyu 5 : 3 pokambilana na anthu za cimene cimapangitsa munthu kukhala wacimwemwe ? Baibulo limatiuza momvekela bwino zimene Yehova ndi Mwana wake , Yesu Kristu , adzacita ndi mavuto amene Satana Mdyelekezi amacititsa . N’ciani cina cingafunike kuti tidziŵe ngati ndifedi munthu wauzimu kapena ayi ? N’zoona kuti si tonse amene tingaciteko upainiya , koma tikhoza kuonjezela nthawi imene timathela mu utumiki wa Yehova . * Citsanzo cina ndi ca Yakobo , amene ananamizidwa kuti mwana wake Yosefe waphedwa ndi cilombo ca kuchile . ( Yobu 31 : 13 - 22 ) Inde , ngakhale pamene anali wochuka ndi wolemela , iye anali wodzicepetsa ndipo anali kulemekeza ena . Ndipo ngakhale ena atinyoze , timakhulupililabe kuti akufa adzauka . — Maliko 12 : 18 ; Mac . 4 : 2 , 3 ; 17 : 32 ; 23 : 6 - 8 . Kuti tidziŵe mmene tingacitile zimenezi , tiyeni tikambilane zitsanzo zina zimene zinacitikadi . Yehova amakamba ndi anthu m’njila yakuti anthuwo asavutike kumva . ( Miy . 1 : 8 , 9 ) Tiyeni tikambitsilane mfundo zitatu za m’Baibo zimene zingakuthandizeni kupanga zosankha zabwino zimene zingakupindulitseni mtsogolo . Komanso angelo sanayambe akhalapo anthu padziko monga makanda , ana , kapena acikulile . Angelo anacita kulengedwa na Yehova . Limapeleka mayankho ogwila mtima a mafunso ofunika kwambili . Koma pitilizani kupempha mzimu , ndipo Yehova adzatembenuzila maganizo anu ku zinthu zoyenela . 16 : 16 ) Panthawiyo , anthu onse amene ali ngati mbuzi “ adzacoka kupita ku ciwonongeko cothelatu . ” Paulo anauza abale a ku Filipi kuti apitilize kupita patsogolo . Komabe , ‘ anasambitsidwa kukhala oyela ’ ndi ‘ kupatulidwa . ’ ( 1 Akor . ( 1 Yohane 2 : 15 , 16 ) Conco aliyense wa ife ayenela kudzifufuza nthawi zonse ndi kuona ngati amakonda zinthu za m’dzikoli . 15 : 26 . ( Afil . 4 : 13 ) Louis anafotokoza kuti : “ Tinaona kuti Yehova anayankha mapemphelo athu potipatsa ‘ mtendele wa Mulungu . ’ Anthu acimwemwe ndi amene . . . N’naona kuti anali na mzimu wopatsa umene Yesu analamula Akhristu kukhala nawo . Atumiki ena a Mulungu amene anacita chimo lalikulu pambuyo pake n’kulapa , amadziimbabe mlandu mpaka kufika poganiza kuti Yehova sadzaiŵala chimo lawo . Zimene io anali kucita zinasonyeza kuti sanaiwale colowa cao , kapena kuti zimene io anaphunzitsidwa . Koma zimenezi zinaonetsa kuti Jairo anali kumva zimene atate anali kukamba . ( Mac . 17 : 18 , 23 - 25 ) Ndipo kumapeto kwa ulendo wake wacitatu wa umishonale , Paulo anacenjeza anthu ochedwa ndi dzina la Mulungu kuti : “ Ndikudziŵa kuti ine ndikacoka , mimbulu yopondeleza idzafika pakati panu ndipo sidzasamalila gulu la nkhosa mwacikondi . Ndipo pakati panu anthu ena adzayamba kulankhula zinthu zopotoka kuti apatutse ophunzila aziwatsatila . ” ( Mac . Iye anati : “ Zinali zovuta kuleka cizoloŵezi cimeneci pambuyo pa zaka zambili . Mosakaikila , inu simufuna “ kumangidwa m’goli ” ndi munthu amene angakucititseni kusiya kutumikila Mulungu . Komabe sititamanda mopambanitsa abale odziŵika kwambili amene amatsogolela mumpingo wacikhristu . Wacicepele wina dzina lake Stephen Miller anaona kuti nchitoyo inafunika kucitika mwamsanga , ndipo anacitapo kanthu . Satana ndi wodzikuza ndiponso wonyada kwambili . ( Yoh . 7 : 16 ; 8 : 28 ) Iye anali kuphunzila Malemba mwakhama kuti aziwagwila mau , kuwateteza , ndi kuwafotokoza bwino . M’nkhani yoyamba tafotokozamo cocitika cina cakale coonetsa kuti wolosela wina wa ku Delphi anasoceletsa mfumu Kolosase , zimene zinacititsa kuti agonjetsedwe na mfumu ya Peresiya . 4 : 8 - 31 . Ayenelanso kuyesetsa kucita zimene Yesu anaphunzitsa . Komabe , pa zifukwa zimene tifotokoze m’nkhani ino na yotsatila , tidzaona kuti kwakhala kofunika kuipendanso nkhaniyi . Kodi zimenezi zinayamba liti kucitika ? Nanga zinacitika bwanji ? ( Deuteronomo 33 : 13 ) Ulaliki wathu ungakhale dalitso , kapena mphatso kwa anthu amene angaulandile . 2 : 5 - 7 . Ndiyeno nkhaniyo imati , cilombo “ cidzazigonjetsa ndi kuzipha . ” 21 : 15 ) Pa moyo wake wonse , Petulo anacitadi zinthu mogwilizana ndi mau ake . ( Ŵelengani Yoswa 23 : 14 . ) Kodi gulu la Yehova lacita zinthu zotani ? Baibulo limati : “ Munthu aliyense adye ndi kumwa ndi kusangalala ndi zinthu zabwino , cifukwa coti wagwila nchito mwakhama . ( Ŵelengani Yohane 17 : 16 . ) Koma ngakhale kuti mafuko 10 a Isiraeli saimila anthu amene adzakhala pa dziko , mgwilizano umene unafotokozedwa mu ulosiwu umatikumbutsa za mgwilizano umene ulipo pakati pa anthu amenewa ndi amene ali na ciyembekezo copita kumwamba . Yehova anakambilatu za kupita patsogolo kumeneku . ( Sal . 34 : 15 ) Mwacitsanzo , ganizilani za Sifira ndi Puwa , anamwino aciisiraeli . Mlongo wa kum’mwela kwa Europe amene tam’tomola kuciyambi kwa nkhani ino , anaphunzila mfundo imeneyi . Pali pano , iwo akutumikila mwacimwemwe m’kagulu ka citundu ca manja mu mzinda wa Mandalay . Tinasangalala kwambili kuti ana athu anasankha kutumikila Yehova . Munthu sangathe kuwapeleka mpaka kale - kale . ” “ Tamvelani , Aisiraeli inu : Yehova Mulungu wathu ndi Yehova mmodzi . ” — DEUTERONOMO 6 : 4 . Yesu anauza ophunzila ake kuti afunika kukhala odzicepetsa ndi kupewa kudzikonda , ndipo anawapatsa citsanzo pa nkhaniyo . Banja lina mumpingo wao linazindikila kuti io afunikila thandizo . Yehova amatilangiza : Yehova amatiphunzitsa , kutitsogolela , ndiponso kutiongolela . Anthu ambili amene timakumana nao muulaliki samaona Mulungu monga bwenzi lao lapamtima ngakhale kuti amakhulupilila kuti iye aliko . Tidzaphunzilanso mmene tingapewele kutengela anthu amene anakana kuona dzanja la Mulungu . Koma nthawi zonse tinali kupempha Yehova kuti atilimbitse ndi kutipatsa nzelu zotithandiza kukhala odzicepetsa n’colinga cakuti zocita zathu zipeleke ulemelelo ku dzina lake lalikulu . Mu June caka ca 1918 , asilikali amene anali ku France anagwidwa ndi mlili woopsa wochedwa Fuluwenza ya ku Spain . 11 : 20 - 22 . 12 : 3 , 4 ) Nthawi ndi nthawi , ziwanda zaonetsa kuti ndi zamphamvu mwa kuvutitsa kwambili anthu amene zawagwila . ( Mat . ( Luka 13 : 1 - 5 ) Iwo anafa osati cifukwa ca khalidwe lao , koma cifukwa cakuti anali munsi mwa nsanja pamene inagwa . Umu ni mmenenso zilili na Mabaibo akale amene anamasulidwa m’zinenelo zina . Inde , Ahabu anadzicepetsa . Iwo anauzidwa kuti : “ Mitundu yonse ya anthu padziko lapansi adzaona kuti mukuchedwa ndi dzina la Yehova , ndipo adzacita nanu mantha . ” ( Deut . ▪ “ Inu Ndinu Mboni Zanga ” ( Oweruza 11 : 1 - 3 ) Yefita sanalole kuti zocita zao zankhanza zim’pangitse kukhala munthu woipa . N’nayambila kuphunzitsako abale anga . Kwa wiki yathunthu , wapolisiyo anaonetsetsa kuti pafupi na nyumba yathu pakukhala apolisi , moti anthu oukilawo sanapitilize kutivutitsa . 22 : 34 - 39 . Kope ya Informant ya mu 1937 , inaika mlingo wa maola 1 miliyoni amene ofalitsa anafunika kukwanilitsa mu 1938 . Kodi munthu afunika kucita ciani kuti ayenelele ubatizo ? Monga mmene mphunzitsi wabwino angathandizile wophunzila wosadziŵa zambili , Yehova nayenso amatithandiza kuti tipite patsogolo mwa kugwilitsila nchito abale ndi alongo athu . Mmishonale uja anawakumbutsa kuti ayenela kuleka kukoka fodya coyamba kuti ayenelele kukhala ofalitsa . Kodi ife timakonda ciani maka - maka mu umoyo wathu ? Sisera anaganiza kuti Yaeli adzalemekeza m’gwilizano wapakati pa mwamuna wake ndi Mfumu Yabini . Nakhala nikuona mmene Yehova watsogolela ndi kudalitsa nchito yolalikila ku Ireland . Kodi ndinu ofunitsitsa kucita ciani ? Nanga tidzakambilana ciani m’nkhani yotsatila ? ( Yoh . 6 : 44 ) Ndipo tingawatsimikizile kuti Yehova amawakonda kwambili atumiki ake a “ mtima wosweka ” kapena “ odzimvela cisoni mumtima mwao . ” ( Sal . Zimenezi zinali zomvetsa cisoni kwambili . “ Kuti akayesedwe ndi Mdyelekezi . ” Tikakumana ndi mavuto aakulu , timazindikila kuti tifunika kudalila Yehova . Koma onani anthu amene tsopano anali nawo paulendowu . Iwo amaiwala kothelatu mfundo za makhalidwe abwino a Yehova . Amasiya kuceza wamba , ndipo amayamba kugwilana manja , kupsopsonana , kusisitana , ndi kugwilanagwilana modzutsa cilakolako . Anthu okhulupilikawo “ anacoka kumbali zonse , ” ndipo sanafune kuika moyo wao pa ngozi . Pali kufanana kotani pakati pa pangano la Cilamulo ndi pangano latsopano ? Safunika kucita kutichulila kuti kavalidwe aka ndiye koyenela , aka n’kosayenela iyai . Pa nthawi imeneyo , onse amene adzaweluzidwa monga nkhosa adzapulumuka , ndipo amene adzaweluzidwa monga mbuzi adzawonongedwa . Baibulo ikanawonongeka , sembe uthenga wake kulibe . Wokwelapo wake dzina lake linali Wokhulupilika ndi Woona . Iwo anauzidwa kuti adzacotsedwa sukulu akakana kucita mwambowo . Kodi ndidzawaonanso atate anga okondedwa kapena mng’ono wanga , Benjamini ? Iye anati : “ Zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inunso muwacitile zomwezo . ” Tifunika kumutamanda cifukwa ali na mphamvu zosayelekezeka , zimene zimaonekela m’zinthu zodabwitsa zimene analenga . N’zoona kuti m’Mabaibulo ena akale kwambili , muli zinthu zina zosiyanako pang’ono . 17 Kodi Muyenela Kusintha Maganizo Anu ? Ndinadziŵa kuti ndifunika mnzanga wogwila naye nchito ya Ufumu . 13 : 14 , 15 ; Eks . 2 : 5 - 10 ) N’zoonekelatu kuti Mose anali kuganizila kwambili za madalitso amene anthu a Mulungu adzalandile . Fotokozelani wophunzila cifukwa cake afunika kucita zimene mwam’pempha , ndipo muyamikileni cifukwa ca khama lake poyesetsa kucita zimenezo . ( Onani ndime 5 mpaka 8 ) Kukamba mofatsa pamene ticita zinthu ndi acibululu amene akutitsutsa kumathandiza . Koma khalidwe lathu labwino , n’limene lingathandize ngako . Timayamikila kwambili kukhala m’gulu la abale amene amakondana ndi kuthandizana ndi mtima wonse . Kukhululukilana kungazimitse mikangano imene ili ngati moto Ngati muona kuti akali wamng’ono cakuti sangapalase njinga , mungafune kuyembekezela . Timalalikila ndi colinga cabwino cifukwa cakuti timakonda Yehova ndiponso anthu ena . Musaiŵale kuti Yesu analangiza otsatila ake kuti : “ Khalani maso , khalani chelu , pakuti simukudziŵa pamene nthawi yoikidwilatu idzafika . M’zocitika zonsezi , taona kuti Yehova anaonetsetsa kuti onse amene anali kum’funafuna anakhala ndi mwai wom’dziŵa . Muzilimbikitsidwa ndi Mphatso ya Mulungu Yosatheka Kuifotokoza , Jan . Kodi mumaphunzitsa mwana wanu kukonda mulungu ? Inanithandiza kukhala wolimba mtima ndi kudalila kwambili Yehova , ” anatelo Zeynep wa ku France . Iye ananiuza kuti : “ Tabwela Sammy , tiye tisangalatsane ! ” ( Yoh . 14 : 26 ) Tikakumana ndi mayeselo , mzimu ungatithandize kukumbukila nkhani za m’Baibo ndi mfundo zimene zingatithandize kusankha mwanzelu . Nditakwanitsa zaka 14 , ndinacokelatu pa nyumba . Juan wa ku Mexico anati : “ Zimenezo zimacititsa onse kukhala omasuka kwambili ndipo amakonzekela nkhani imene tidzakambilana . ” ( b ) Fotokozani zitsanzo za cikondi cacinyengo . Pa Miyambo 5 : 8 pamati : “ Njila yako ikhale kutali ndi [ mkazi waciwelewele ] . Mavuto a zacuma , matenda , ndi mavuto ena zingacepetse cikondi ndi ulemu m’banja lao . Conco , mwamunayo ndi mkazi wake anagwilitsila nchito ambulela imodzi , ndi kupatsa mwininyumba ambulela inayo . Komanso , mungawathandize kudziŵa mmene angafikile anthu polalikila uthenga wa Ufumu m’gawo lanu . Masiku ano , akapolo amaseŵenza m’migodi , kugwila nchito yoŵaŵa koma yamalipilo ocepa , ndi kuumba nchelwa . Mwapemphelo onani ngati mungasinthe zinthu zina kuti mutengeko mbali pa nchito yosangalatsa imeneyi ku New York kapena panchito zina zomanga , ndipo mudzaona mmene Yehova adzakudalitsilani . — Maliko 10 : 29 , 30 . Koma kodi ucimo unali ciani ? Nanga unatsogolela bwanji ku imfa ? Anakamba kuti tiyenela kuseŵenzetsa ufulu wathu “ monga akapolo a Mulungu . ” Komabe , sindinali kudziŵa tanthauzo la pemphelo limeneli mpaka nditakwanitsa zaka 20 . Masiku ano , m’Nyumba za Ufumu zambili muli masikilini amene amaonetselapo mau a m’nyimbo . Ni pemphelo la mau oonetsa cikhulupililo , acitamando , ndi oyamikila . — 1 Sam . M’buku la Genesis , muli macaputa okwana 15 okamba za Abulahamu . 1 : 7 - 9 . Zimenezi zinatha . Posacedwapa , “ dziko lapansi lidzadzaza ndi anthu odziŵa Yehova ngati mmene madzi amadzazila nyanja . ” — Yesaya 11 : 9 . Pa tsiku lacitatu , iye anaukitsa Mwana wake , ndipo pa tsiku la Pentecosite wa mu 33 C.E . , Yesu anakhazikitsa ufumu wauzimu pa mpingo wacikristu wa abale ake odzozedwa . ( Akol . ( a ) Kodi citanthauza ciani tikanena kuti lonjezo lanu la kudzipeleka kwa Yehova n’losasinthika ? Yehova afuna kuti atumiki ake azigwilizana ndi kukhala ndi colinga cimodzi Nthawi zambili Paulo anali kuzunzidwa cifukwa ca kukhulupilika kwake . ( 2 Akor . Citsanzo cabwino ca makolo athu ndiponso zimene anali kutiphunzitsa , zinatithandiza anafe kuti tiyambe kukonda Mulungu . Pali mitundu inayi ya cikondi . ( b ) Kodi timamvela bwanji tikaona anthu amene anadzipeleka akubatizika ? Conco “ zinthuzo zinali zokwanila pa nchito yonse yoyenela kucitika , ndipo zinaposanso zinthu zofunikila pa nchitoyo . ” — Eks 35 : 21 - 24 , 27 - 29 ; 36 : 7 . Kodi mumada nkhawa cifukwa coopa kukalamba ndi kukumana ndi mavuto amene amabwela cifukwa ca ukalamba ? 6 : 22 ) Mwa ici , Nowa na banja lake anapulumuka ciwonongeko ca dziko la pa nthawiyo . — Aheb . Ndipo kumbukilani kuti Yehova angatithandize kukhala na makhalidwe amene angatithandize kupanga zosankha mogwilizana ndi cifunilo cake . Mwina mungacepetseko nthawi yogwila nchito ndi yocita zinthu zina kuti muzikhala ndi nthawi yambili yoceza ndi ana anu . Tingapemphe ofalitsa atsopano kuti atipelekeze ku maulendo obwelelako kapena kukatsogoza maphunzilo a Baibulo . 4 : 14 . Iye anakamba kuti izi sizingatheke mwa nzelu zathu cabe . Cinthu cina cofunika kwambili ni citsanzo canu . Zimalemekeza maboma olamulila koma zimakhulupilila kuti ndi Ufumu wa Mulungu wokha umene ukhoza kuthetsa mavuto onse a mtundu wa anthu . ” — Anatelo Nová Svoboda , wofalitsa nkhani ku Czech Republic . ( 2 Akorinto 2 : 17 ) Ophunzila a Yesu sayenela kuuza anthu kuti awalipile cifukwa ca nchito yao yolalikila . 19 : ​ 7 - 9 ) Aliyense amene adzakhala ndi moyo padziko lapansi adzapindula ndi cikwati ca kumwamba cimeneco , cifukwa cikwatico ndi citsimikizo ca boma labwino . Ana athu amadziŵa kusiyanitsa cabwino na coipa . Kuganizila zinthu zimenezi kungatithandize kuyamikila kwambili dipo — mphatso ya Mulungu yopambana zonse . Coonadi conena za Ufumu wa Mulungu cili ngati ngale yamtengo wapatali . George , amene nyumba yake inawonongekelatu mumzinda wa Tacloban , anati : “ Mosasamala kanthu na zimene zinacitika , abale ni osangalala . Popeza anali wacicepele , mwina poyamba Timoteyo anali kudzikayikila na kuyopa kucita zinthu monga mwamuna wa pa udindo . ( 1 Tim . Izi ni zimene Ulf anacita . Kodi kuceza ndi anthu oipa kungakhudze bwanji moyo wathu ? Iwe ndiwe mwana kwambili poyelekezela na ine , koma waniphunzitsa cinthu cofunika kwambili mu umoyo wanga . ’ Ngati titsatila zimene tiphunzila m’Baibulo , tingasankhe zinthu zimene zingakondweletse Yehova . Kukhala ndi mzimu wodzimana kudzakuthandizani kulandila thandizo la akulu . Ngakhale kuti udindo unaonjezeka wolela ana , tinaganiza zakuti ndiyambe upainiya wanthawi zonse . Iye amaonetsa cikondi kwa ana ake mwa kufotokoza momveka bwino malamulo ndi mavuto amene angakhalepo ngati sanamvele malamulowo . Mkulu wa ophika mkate ataona kuti Yosefe wamasulila zabwino pa loto la wopelekela cikho , nayenso anapempha Yosefe kuti amasulile loto lake . Mkulu wa ophika mkateyo anakamba kuti anaona mbalame zikudya mkate umene unali munsengwa zitatu zimene zinali pa mutu pake . Kodi mtima wapacala unganibweletsele mavuto anji ? Vuto limene lilipo ndi lakuti akukumana ndi zinthu zimene zikumucititsa kuona kuti kutsatila zimene mumakhulupilila n’kovuta . ” Ngakhale mbalame zapeza malo okhala pafupi ndi guwa lanu lansembe lalikulu . Namzeze wadzimangila cisa cake pamenepo , ndi kuikamo ana ake ! ” Liu la Cigiriki limene linamasulidwa kuti “ anamuneneza , ” pa Luka 16 : 1 , lingatanthauze kuti mtumikiyu anamunamizila . 8 : 13 ) Zimenezo zitacitika , Mulungu anayamba kuona Ayuda ndi anthu Akunja osadulidwa mofanana , cifukwa cakuti ‘ mdulidwe wao ndi wa mumtima wocitidwa ndi mzimu , osati ndi malamulo olembedwa . ’ 3 : 3 ) Munthu wolapa ndiye ayenela kucitilidwa cifundo . ( Genesis 1 : 28 ) Conco lamulo limeneli linali loletsa mtengo weniweni . Koma Yesu sali mbali ya pangano latsopano . Zimenezi zinacitikadi . Abale ndi alongo mumpingo wanu angakuthandizeni kupewa kutenga mbali m’zandale . WOPEKA nyimbo wina anati : “ Mau okambidwa amacititsa munthu kuganiza . Kusinkhasinkha mmene Yehova wationetsela cikondi kudzatithandiza kulimbitsa ubwenzi wathu ndi iye . Koma kodi ndeke zingaikile mazila na kukonkhomola tuŵana twa ndeke ? Anapatsidwa masiku osiyana - siyana okhala m’ndende kuyambila pa masiku 45 mpaka miyezi 5 ndi hafu . Naye mwamuna wake , Fred , anati : “ N’nali kale ndi vuto lopanga zosankha . Kodi io anatengelako ucimo ndi imfa ? Pa cifukwa cimeneci , Yesu anauza anthu amene anali kulankhula nao kuti : “ Mvelani kuno nonsenu , ndipo mumvetse tanthauzo lake . ” — Maliko 7 : 14 . Anthu ena amacita ciliconse cimene aganiza . Pitilizani kupempha Ufumu wa Mulungu kuti udzayeletse dzina lake ndi kupangitsa cifunilo cake kucitika pa dziko lapansi . N’cifukwa ciani tifunika kupewelatu kucita zinthu modzikweza ? ( b ) Tingatengele bwanji citsanzo ca Yesu ? Iye anali kunena mofuula kuti : ‘ Opani Mulungu ndi kumupatsa ulemelelo , cifukwa ola lakuti apeleke ciweluzo lafika . Monga mmene lembali lasonyezela , Mose , Aroni , ndi Samueli anacilikiza mokwanila makonzedwe a kulambila koona . ( Sal . Kugwila nchito ya Yehova nthawi zonse , kumatithandiza kuikabe maganizo athu pa nkhani yaikulu yokhudza ucifumu wa Mulungu . Zinali zokhumudwitsa kuona kuti ana ena amaleka kutumikila Yehova ngakhale kuti pali zitsanzo zabwino kwambili zimene angatengele . Nthawi zambili thilaki yawo ikawonongeka , anali kuyenda wapansi kapena kucova njinga kupita m’tauni yapafupi . Nanga bwanji za anthu mamiliyoni osalakwa amene anafa pangozi ? ( Yer . 15 : 16 ) Yeremiya anadya mau amtengo wapatali a Mulungu mophiphilitsila mwa kuwasinkhasinkha . Atandipatsa ndinayamba kuliŵelenga , ndipo ndinapezamo kapepala ka uthenga kosindikizidwa ndi Mboni za Yehova kamene Rudi anaikamo . Malinga ndi buku lina , liu la Cigiriki lomasulilidwa kuti ‘ kubangula ’ limanena za “ kulila kwa cilombo ca njala kwambili . ” ( Ŵelengani Miyambo 12 : 18 . ) Wandilola kuti ndim’dziŵe ndi kum’tumikila . Wandipatsanso mwamuna wabwino amene amakonda Yehova . Cinanso , kumbukilani kuti kuphunzitsa kozikidwa pa malemba sikutanthauza kungoŵelenga malemba ambili . Maka - maka zimene zimaikila pansi monga nkhuku , zimakhala chelu kwambili kuyang’ana adani . N’ciani cimene tiyenela kuika pambali ? Don atamva zimenezo , mwanzelu anaseŵenzetsa malemba atatu poyankha Peter momufika pamtima . 110 : 3 . Rehobowamu anaona kuti zinali zovuta kupanga cosankha pa nkhaniyi . Kuti zimenezi zitheke , Mulungu anatipatsa Baibo kuti izititsogolela . Ŵelengani Salimo 45 : 13 , 14a . ( Mac . 10 : 42 ) Mwacitsanzo , anthu ocilikiza Ufumu okwana pafupi - fupi 20,000 anasonkhana pa msonkhano waukulu wa mayiko ku Cedar Point , Ohio , U.S.A . , mu September 1922 . Covala cimeneco cinali kuvalidwa ndi anthu olemekezeka kapena mafumu . [ 1 ] ( ndime 7 ) Zina mwa mfundo zimene Yesu anaphunzitsa ni ( 1 ) Kulalikila uthenga woyenela . M’pemphelo la citsanzo , Yesu anapempha Mulungu cinthu caciŵili . Anati : “ Ufumu wanu ubwele . ” ( c ) kuthetsa mikangano ? N’zomvetsa cisoni kuti anthu ena a Mulungu ayamba kutengela “ mzimu wa dziko . ” Mwa ici , iwo sasiyana kweni - kweni ndi anthu ‘ amene satumikila Mulungu . ’ ( 1 Akor . Iye anati : “ N’nali n’tadziikila kale colinga cocita upainiya pamene n’nali mwana . Monga Tate wacikondi , anali kufuna kuniteteza ku ngozi imene imabwela cifukwa cotamba zamalisece . M’fanizo limeneli , Yesu sanachule mwacindunji kuti zipatso zimenezi n’ciani . Koma anakamba mfundo inayake yofunika imene ingatithandize kupeza yankho . Kutsatila citsanzo ca Abulahamu kungatithandize bwanji kupitilizabe kutumikila Mulungu ? Kuwonjezela apo , tifunikanso kulimbana ndi zofooka zathu ndi zinthu zina zokhumudwitsa . — 2 Akor . Mwa kuseŵezetsa mavesi a m’Baibulo , ananithandiza kudziŵa mmene ningathetsele zizoloŵezi zanga . Iye ananilimbikitsanso kuti nizipempha thandizo kwa Yehova nthawi zonse . — Salimo 119 : 37 . Munthu wacikulile amene anali kutsogolela anali kulidziŵa bwino dzikoli . Muzifunafuna malangizo a m’Malemba Ndipo mwacionekele , dzina limeneli limatanthauza kuti , “ Iye Amacititsa Kukhala , ” kuonetsa kuti ali na mphamvu zokwanitsa kudziŵa na kuonelatu zocitika zam’tsogolo mogwilizana na cifunilo cake . Eduardo anati : “ Kwa zaka ziŵili zoyamba tinalibe ndalama zokwanila . 2 : 11 - 14 ) Ifenso tikaona kuti tili na maganizo aliwonse a tsankho , kapena onyadila mtundu wathu , tifunika kuyesetsa kuwanyula mumtima mwathu . Kumbukilani mmene Mose anayankhila pamene amuna ena mu msasa wa Aisiraeli anayamba kucita zinthu monga aneneli . 1 : 27 ) M’Baibo muli zitsanzo zambili za anthu amene anaonetsa khalidwe la cifundo . Ndinapemphelanso kwa Yehova ndi mtima wonse ndipo ndinapita kukafuna nchito . Zozizwitsa za Yesu zimaonetsa kuti iye amatikonda ndiponso amakhudzidwa ndi mavuto athu ( Onani ndime 11 ndi 12 ) Mukatelo , mumaonetsa kuti mumanyadila kudziŵika ndi dzina la Yehova , ngakhale kuti ena angakusekeni . 6 : 25 - 33 ) Popeza kuti Mulungu amatikonda ndi kutisamalila , tiyenela kucita zonse zimene tingathe kuti tikondweletse mtima wake . — Miy . 3 , 4 . ( a ) Ndi kuti kumene tingapeze Tetragalamatoni ? Kodi kuganizila za mafumu anayi amene takambilana kungakupindulitseni bwanji ? Anapezanso cimwemwe cimene cimabwela cifukwa cokhala wopatsa mwa kuuzako ena zimene anaphunzila . Damaris anaphasa bwino kwambili mayeso a ku sekondale . Paulo anali kudziŵa kuti anthu oona mtima komanso odzipeleka pa zinthu zabwino , angathe kusintha n’kukhala otsatila a Khristu acangu . Mu 1919 , io pamodzi ndi odzozedwa ena anaikidwa kukhala “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” kuti asamalile zosoŵa za kuuzimu za anthu a Mulungu m’masiku otsiliza . — Mat . ( Aroma 7 : 5 ) Izi zitithandiza kumvetsa mau a Paulo akuti anthu “ otsatila zofuna za thupi amaika maganizo awo pa zinthu za thupi . ” Tinene kuti munthu wina wakutumilani foni , koma simunam’zindikile . Popeza taona kuti ubatizo ni wofunika kwambili , tiyeni tikambilane mafunso atatu awa : Kodi Baibo imakamba ciani za ubatizo ? Wansembeyo anauza Kolosase kuti adzagonjetsa “ ufumu wamphamvu . ” KUONONGEDWA KWA MABOMA A ANTHU . 11 : 27 . Nthawi . ( Yohane 15 : 15 ) N’zoona kuti Yesu nthawi zina anali kukhala yekha kuti apeze nthawi yosinkhasinkha ndi kupemphela . Kodi Mkhiristu angacite ciani kuti akhale na umoyo wosalila zambili ? 4 : 20 ) Ndiyeno tiyelekezele kuti mlongo , amene mwamuna wake ndi wosakhulupilila , wakonza zakuti apite mu ulaliki . Okwatilana amene amalemekezana , amacita zinthu moganizilana olo pamene asemphana maganizo . Ngati mumayesetsa kutumikila modzicepetsa mumpingo , mudzadalitsidwa cifukwa anthu amene amakonda Yehova adzakukondani , kukuyamikilani , ndi kukuthandizani . Baibulo limafotokoza zinthu zitatu zimene zimacititsa imfa . — Mlaliki 9 : 11 ; Yohane 8 : 44 ; Aroma 5 : 12 . Mwacitanzo , ku South Africa , Mboni zambili zimakhala m’madela amene anagaŵidwa motengela mtundu wawo . Ena amakhala m’mayadi , ena m’makomboni a anthu akuda , ndipo ena amakhala m’madela amene kale munali kukhala anthu a mitundu yosiyanasiyana . Kucita izi kudzakuthandizani kukumbukila zimene mwaphunzila . Nanga n’cifukwa n’ciani ? Anthu ambili a Yehova amadzipeleka moona mtima pom’lambila . N’zoona kuti , cifukwa ca cisoni , zingakhale zovuta kufotokoza bwino - bwino maganizo anu popemphela . Komabe , kupemphela naye mocokela pansi pamtima kungamutonthoze kwambili , ngakhale m’takhala kuti mukulila ndipo mau anu sakumveka bwino . Kodi Mulungu adzathetsa bwanji umphawi padzikoli ? — Mateyu 6 : 9 , 10 . Mfundo zisanu zimene tafotokoza zidzakuthandizani kuti muyambe kuŵelenga Baibo . Cikondi na kukoma mtima zingatilimbikitse kukhululukila ena . Koma Yehova sangacitile ana ake zimenezo . Kodi ndi zocitika ziti zimene Akristu acinyamata ambili akusangalala nazo ? Zimene zakhala zikucitika pakati pa anthu a Mulungu zimasonyeza kuti mapeto ayandikila . Wosimba ni Felix Fajardo Zinali kuoneka ngati ulemelelo wa Yehova . ” — Ezekieli 1 : 27 , 28 . Iye anawauza kuti : “ Musaope ayi . Pali nkhani zina zimene Baibulo silipeleka lamulo mwacindunji . M’malomwake , ndinayamba kufooka mwakuuzimu . A Zulu : Conco caka ca 607 B.C.E . cinali ciyambi ca nthawi zokwanila 7 , kapena nyengo ya nthawi pamene ulamulilo wa Mulungu unasokonezedwa . Mwacitsanzo , ena anafunsa ngati kunali kwa phindu kupitiliza kutulutsa zofalitsa m’Cituvalu . Nanga mungamamve bwanji mukaganizila kuti simunamvele malangizo opindulitsa amene Mulungu anakupatsani ? ( Yuda 22 , 23 ) Ngati ndinu mwana wa sukulu , ndipo aphunzitsi anu akuphunzitsa za cisinthiko , limbani mtima ndi kuteteza cikhulupililo canu pa nkhani ya cilengedwe . Akatswili a mbili yakale amacitila umboni kuti Koresi anaonongadi mzinda wa Babulo . Kodi nthawi zonse nimapempha Yehova kuti asanthule mtima na malingalilo anga ? Pamene tipitiliza kuphunzila za Yehova ndi kumumvela , iye adzatidalitsa ndi kutiteteza . 11 : 13 . 1 : 27 , 28 ; 2 Tim . Pamene ena mwa angelowo anakopeka na kubwela pa dziko lapansi kudzacita ciwelewele na akazi , akaziwo anabala vimphona vimene vinayamba kupondeleza mtundu wa anthu . ( Gen . Nanga iwo anasankha ciani ? Mbadwa za a Adamu zinatengela ucimo ndi imfa kwa makolo awo osamvela . Pokamba nkhani ya anthu onse , m’patseni autilaini ndi kumuuza kuti azikutsatilani n’colinga cakuti aone mmene mukufutukulila mfundo . Coyamba , onani maganizo amene munthu wakuthupi amakhala nawo . M’masiku amenewo n’naphunzila kuti kupatsa kumabweletsa cimwemwe . — Mat . Tikaŵelenga nkhani yokamba za cilengedwe m’buku ya m’Baibo ya Genesis , timaphunzila kuti Mulungu anauza munthu woyamba , Adamu , kuti : “ Zipatso za mtengo uliwonse wa m’mundamu uzidya ndithu . Phunzilani zimene mungacite kuti mudzakhale m’dziko lopanda nkhanza Anthu amene ali na cizoloŵezi cotamba zamalisece , amakhala ndi “ cilakolako ca kugonana ” cosaletseka , moti nthawi zonse amalaka - laka kucita ciwelewele . Inenso zinanditengela nthawi kuti ndimvetse maulosi amenewa ndi kukwanilitsidwa kwake . Mwacitsanzo , taganizilani za Gavin . Kodi Cikumbumtima Canu n’Codalilika ? Akulu amene ali ndi udindo wofotokozela munthu cigamulo cakuti wacotsedwa ayenela kucita zinthu mwacikondi monga mmene Yehova amacitila . Kukhala na colinga cimeneci kungakhale kwabwino kwambili , cifukwa mphatsoyo ingathandize woilandila na kukondweletsa woipeleka . Ndiponso , dziikile colinga coŵelenga Baibulo yonse . Tizilalikila mwacangu “ coonadi ca uthenga wabwino ” kwa ena . 39 : 20 - 23 ) Citsanzo ni M’bale Harold King , amene anapika jele kwa zaka zambili cifukwa ca cikhulupililo cake . CAPAKATI pa zaka za m’ma 1930 , atate anga a James Sinclair ndi amayi , a Jessie Sinclair , anasamukila m’dela la Bronx , mumzinda wa New York . Zinthu zimenezi zimaphatikizapo kuceza ndi banja lathu ndiponso mabwenzi athu . Komabe , iwo ali ndi ufulu ndi udindo wodzipangila zosankha . Mwacitsanzo , nthawi zambili okalamba amakonda kuceza ndi a m’banja lawo . M’bale Guy Pierce anabadwa pa November 6 , 1934 ku Auburn , m’dela la California , m’dziko la United States , ndipo anabatizidwa mu 1955 . Iye anafotokoza kuti “ munthu wakuthupi salandila zinthu za mzimu wa Mulungu , cifukwa amaziona ngati zopusa ndipo sangathe kuzidziŵa . ” ( b ) Pelekani citsanzo coonetsa mmene kuunjika cuma cakuthupi kumasiyanilana ndi kuunjika cuma ca kuuzimu . Aiguputo anali kukhulupilila kwambili maloto , ndipo anali kudalila kwambili anthu amene anali kudzicha omasulila maloto . Kucokela panthawiyo , mwa cisomo ca Yehova , anthu ake akhala akukula m’cidziŵitso pa cifunilo ca Mulungu , ndi m’cikondi cawo kwa Atate wawo wakumwamba . Pamenepa pali cigawo cakuti “ Mabuku . ” Pa cigawo cimeneci pali zofalitsa zambili zothandiza . 11 : 29 ) Iye anali kucita zinthu moleza mtima kwambili ndi otsatila ake ngakhale kuti iwo anali kulakwitsa zinthu zina . 12 : 25 ; Akol . 4 : 11 ) Tikacita zimenezi , timaonetsa mwa zokamba ndi zocita zathu kuti timakondadi “ abale ndi alongo athu m’cikhulupililo . ” — Agal . Ngati mophiphilitsila tiikabe maso athu pa Yehova , sitidzalola zocita za ena kutikhumudwitsa kapena kuticititsa kuwononga ubwenzi wathu na iye . ( Eks . 12 : 49 ; Lev . Motelo , tinawafunsa kuti : “ N’cifukwa ciani Akristu amalambila Yesu , mtanda , Mariya , ndi mafano pamene kucita zimenezi ndi kosemphana ndi Malamulo Khumi ? ” Makolo a wacicepele wa zaka 15 ku South Africa anati : “ Mwana wathu akangolandila Galamukani ! Koma zinali zotheka kwa Yesaya ndipo timvetsetsa mmene iye anamvelela . Nakhala na mwayi wamtengo wapatali wocezela abale m’maiko oposa 90 2 : 22 . 3 : 8 ) Kodi Satana anaganizilapo zoti kupha khanda ndi kucita zinthu mopitilila malile ? ( Salimo 49 : 6 - 9 ) Popeza kuti Yesu sanatengele ucimo ulionse , iye anali wangwilo mofanana ndi Adamu . Patapita nthawi , Rubeni mwana woyamba wa Yakobo anagona ndi Biliha mkazi wacinai wa atate ake , ndiyeno anacititsa manyazi atate ake ndipo mwacionekele anataya mwai wokhala mwana woyamba kubadwa kapena wamkulu . — Genesis 35 : 22 ; 49 : 3 , 4 . Kodi kuyang’ana kwa Yehova kumaphatizikizapo kucita ciani ? Komanso Mulungu wandidalitsa ndapeza mkazi wabwino ndi wokhulupilika , dzina lake Anita . Ambili amayesetsa kuthela maola 70 mu ulaliki mwezi uliwonse . Nthawi imeneyo panali ophunzila okwanila 120 amene anasonkhana ku Yerusalemu , ndipo “ mwadzidzidzi kumwamba kunamveka mkokomo ngati wa mphepo yamphamvu , ndipo unadzaza m’nyumba yonse . ” Pasanapite nthawi yaitali Yosefe analota maloto aŵili odabwitsa . Tingawakumbutse kuti Yehova anawakokela kwa Mwana wake , ndipo ndi amtengo wapatali kwa iye . Thandizo la mabwenzi anga apamtima ndi la abale auzimu , n’lofunika ngako pa nthawi zovuta . Ndinamuyamikila kwambili kaamba ka khama lake ndipo ndinam’pempha kuti ndimve mmene akuŵelengela . Tikatelo tidzakhala ndi cidziŵitso . Conco n’nafunsa a dokota kuti , ‘ Kodi ningapite kukakhala ku Myanmar mosasamala kanthu za vuto langali ? ’ Muzikhala okonzeka . KUKULA KWANGA : Pamene ndinali mwana kwambili , banja langa linali kukhala pafupi ndi mzinda wa Leipzig , Kum’mawa kwa Germany capafupi ndi malile a mayiko a Czechoslovakia ndi Poland . Yesu anati : ‘ Ciliconse cimene mungapemphe Atate m’dzina langa adzakupatsani . ’ ( Yoh . Buku limene iye anakamba n’dzaliŵelenga , cifukwa cimene m’bale wanga angalandile , ciyenela kukhala capadela . ” 5 : 16 - 18 ) Komanso , tikakhala na cimwemwe ceni - ceni , timapewa umoyo wokonda zinthu zakuthupi . Tsopano onani malangizo awa ocokela m’Baibulo amene angakuthandizeni kukhala wosangalala ndi nchito yanu . ( 2 ) Kodi tingaphunzile ciani kwa atumiki a Mulungu amene iye anawapatsapo cilango m’nthawi yakale ? Kodi makolo angatengele bwanji citsanzo ca Yesu pophunzitsa ? Mpaka pano sitipemphetsa ndalama . Tiyeni tizionetsa kuti timayamikila ufulu umenewu mwa zosankha zimene timapanga . Ricky , woyang’anila nchito yomanga ku Hawaii , anaitanidwa kuti athandize panchito yomanga likulu ku Warwick , monga wanchito amene amayendela . Maulendo amenewa anan’thandiza kupitiliza kuona zinthu moyenela . Anan’thandizanso kuona mmene Yehova amakondela anthu a mitundu yonse . — Mac . Pambuyo poukitsidwa , iye analankhula ndi ophunzila ake aŵili amene anali paulendo wopita ku Emau , ndipo ‘ anawatanthauzila zinthu zokhudza iyeyo m’Malemba onse . ’ ADZAOCHA MAFUPA A ANTHU : Kodi ndani akanalosela ndendende za makolo amene anali kudzabeleka mwana amene anali kudzaocha mafupa a anthu pa guwa la nsembe ? Ndani akanalosela za tauni kumene guwa la nsembe linali kudzamangidwila zaka 300 zimenezi zisanacitike ? Machalichi aonjezela msokonezo umenewu mwa kulimbikitsa anthu kugwilitsila nchito Mabaibulo amene dzina la Mulungu lakuti Yehova lacotsedwamo . ( a ) Kodi munthu ‘ angazinyenge bwanji ndi maganizo onama ’ ? Kuganizila mmene atumiki a Yehova akale anali kufotokozela maganizo ao kwa Mulungu kungatithandize kupeleka mapemphelo atanthauzo . 11,163,934 Komanso , kodi ndife otsimikiza mtima kupewanso macimo amene anthu ena angawaone ngati ni aang’ono ? — Aroma 6 : 14 , 17 . 3 : 20 ) Komanso ni Yohane cabe amene analemba kuti , “ Mulungu ndiye cikondi . ” Yamba wadziŵa zimene amakhulupilila . ( 1 Akor . 6 : 18 ) Ciwelewele cacititsa kuti matenda opatsilana pogonana afalikile , ndipo matendawa abweletsa mavuto ambili kuphatikizapo imfa . Coyamba , nimawayamikila anthu aconco cifukwa cokhulupilila Mulungu . Ndiyeno nimawaonetsa zimene Baibo imakamba zosonyeza kuti Yehova ni wacikondi . Nimawafotokozelanso zimene iye walonjeza . ” Ifenso tiyenela kumumvela cifukwa posacedwapa adzaononga dziko loipali . Cofunika ni kuika zinthu za kuuzimu patsogolo mu umoyo wathu . ( b ) Kodi Sakura anali na khalidwe lanji poyamba ? Nanga n’ciani cinamuthandiza kusintha ? Mofananamo muyenela kukonzekela zinthu zimene zidzacitika mogwilizana ndi ulosi wa m’Baibulo . Ngakhale patapita zaka 430 pambuyo popeleka lonjezolo , Yehova sanasinthe colinga cake . — Genesis 12 : 1 , 2 , 7 ; Ekisodo 12 : 40 , 41 . Kayafa anatuma asilikali kuti akagwile Yesu usiku . Yesu anali kudziŵa za ciwembu cimeneci . Atalenga dziko lapansi lokongola , iye analenganso munthu woyamba , Adamu , m’cifanizilo cake . ( Gen . Khalani na colinga . Nthawi imeneyo , ndinayamba kuona kuti ndikutumikila kumalo osoŵa . Mulungu anauza Kaini kuti agonjetse ucimo umene unali ‘ utamyata pakhomo kumudikilila . ’ Mosakaikila , mungakhumudwe kwambili . Kwa zaka zambili , machalichi akhala akuphunzitsa ciphunzitso ca utatu , kuonetsa kuti Atate ndi Mwana ndi cinthu cimodzi cogwilana . Kumbukilani kuti nthawi zina macenjela a Satana amakhala oonekelatu . Muyenela kulimbikitsana ndi mnzanu amene muli naye mu ulaliki , kukhala ndi ndandanda yophunzila Baibulo , kugwilitsila nchito malangizo ocokela kwa kapolo wokhulupilika , ndi kukhala ndi zolinga zoyenela . ( Dan . 11 : 44 , 45 ) Zimenezi zimagwilizana ndi zimene buku la Ezekieli limanena zokhudza Gogi . — Ezek . M’nkhani ino , tidzakambilana umboni woonetsa kuti Yehova , Mulungu wamtendele , ni wadongosolo kupambana wina aliyense . Ngakhale kuti mwina munabatizika posacedwapa mumadziŵa zambili paumoyo . ( Mlaliki 9 : 5 ) Mboniyo inam’thandiza kudziŵa kuti makolo ake akale amene anamwalila sakuzunzika m’moto wa ku helo , koma ali gone m’manda akuyembekeza kuukitsidwa . Iye anati : “ Aliyense acite mogwilizana ndi mmene watsimikizila mumtima mwake , osati monyinyilika kapena mokakamizika , cifukwa Mulungu amakonda munthu wopeleka mokondwela . ” Koma iwo anakana kwamtu wagalu . Conco , tsankho lokhala ngati nguwe limene n’nali nalo na cidani , zinasungunukilatu . ” Kusintha kwa khungu . Kevin anacita zonse zimene akanatha kuti azilamulila mkwiyo wake . Maiyo anati : “ Makolo athu anali kulambila m’phili ili , koma anthu inu mumanena kuti Yerusalemu ndiwo malo kumene anthu ayenela kulambililako . ” — Yohane 4 : 5 - 9 , 20 . Koma mwadzidzidzi zinthu zinasintha . “ Ngati umakonda mnzako , suika kwambili maganizo ako pa zimene amalakwitsa , koma umaona zimene amacita poyesetsa kukhala munthu wabwino . ” — Aaron . Sitiyenela kudandaula cifukwa ca zofooka zazing’ono za anzathu pamene ife tili ndi zazikulu kwambili . NJILA YAPADELA YOONETSELA ENA CIKONDI N’cifukwa cakuti munthu aliyense wodzipeleka kwa Yehova anamulonjeza kukhala wokhulupilika , womvela ndiponso kumukonda . Nthawi zambili timaonetsa Khalidwe Lopambana kwa Akristu anzathu . Mwacionekele , tikanamva zinthu zambili zoipa kuposa zimene tamvapo kale . Kodi cikondi ca Yehova cimaonekela bwanji ndi mmene analengela anthu ? Abale athu , ngakhale osauka kwambili , ali ngati Akhristu a ku Makedoniya . Pamene mavuto akuculukila - culukila , tifunika kulimbitsa kwambili cikondi cathu pa abale na alongo athu . Anthu mamiliyoni amafa caka ciliconse cifukwa ca matenda obwela kaamba ka kucepelekela kwa cakudya . Kale , nthawi imene padziko panali anthu aŵili cabe ( komanso Cigumula citatha , pamene kunali anthu 8 cabe ) , Yehova analamula kuti : “ Mubelekane , muculuke . ” ( Gen . * Kuwonjezala apo , wacifwamba amene ni waukali akaona kuti munthu ali na mfuti , zinthu zingafike poipa kwambili cakuti wina akhoza kuphedwa . ( Aheb . 10 : 38 , 39 ) Tiyeni tiphunzile mmene nkhani yokhudza Mose yopezeka pa Aheberi 11 : 24 - 26 ingatithandizile kulimbitsa cikhulupililo cathu . Pangano la mu Edeni limaonetsa kuti Mulungu adzagwilitsila nchito Ufumu kuti akwanilitse cifunilo cake ca dziko lapansi ndi ca anthu . Comvetsa cisoni n’cakuti , nthaŵi zambili timamumangilila manja ndi miyendo yake pa njinga ya olemala kuti asavulale kapena kuvulaza ena . Ndende ya Yíaros inali yaikulu , yomangidwa na nchelwa zotentha , ndipo munali kukhala akaidi oposa 5,000 amene anamangidwa pa zifukwa zandale . Kodi zitsanzo za mkazi wamasiye wosauka , Eliya , ndi wolemba Salimo 102 , zingatithandize bwanji kukhala ndi maganizo oyenela ? Koma tiyenela kusamala na ma Baibo ena . Tiyeni tikambilanenso citsanzo cina : Mwina mumakonda kwambili zovala za sitaelo inayake , koma mudziŵa kuti ena mumpingo angakhumudwe ngati mwavala zovalazo . Lomba nimakhala wokondwela m’banja ndipo tili na zolinga zabwino pa umoyo . ” N’ciani cimene sitiyenela kuiwala ponena za kupita patsogolo kwa wophunzila Baibulo ? N’kulakwa Mkristu wa Mboni za Yehova amene sali pabanja kukhala pacibwenzi ndi munthu amene si Mboni , ndiponso amene salemekeza miyezo yapamwamba ya Mulungu . Baibo imapeleka zifukwa zomveka bwino zoonetsa kuti Yehova ni woyeneladi kulamulila . 4 : 6 . Baibulo limakamba mosapita m’mbali za khalidwe limene tifunika kuonetsa pamene mapeto akuyandikila . Koposa zonse , kodi Yehova angamve bwanji pa zimene mungasankhe kucita ? — Miy . * Ndiponso muziceza ndi ena amene akhala muutumiki wa nthawi zonse kwanthawi yaitali . Popemphela kwa Atate wake wakumwamba Yesu anapeleka citsanzo coti tizitsatila Atatu mwa anthu okwela pa mahachi amenewa amaimila masoka amene Yesu analosela . Masoka amenewo ndi nkhondo , njala ndi milili . Naye mwana wanu angafotokoze mmene kunalili kovuta panthawiyo kukhulupilila kuti cinthu cacikulu monga dziko lapansi cingalenjekeke m’malele popanda kanthu . ( c ) Kodi colinga ca M’bale Knorr cinali ciani ? Zimenezi zatheka cifukwa Mulungu ndi anzake acikristu amamulimbikitsa . Tikuyamikila acinyamata onse amene amapewa mzimu wa dziko ndi kuyesetsa kutumikila Mulungu mogwilizana ndi abale ndi alongo onse . Nthawi zina , mungakumane ndi mavuto amene angacititse kuti mukhale na nkhawa kwambili . Ife anthu timamvetsetsa mmene olemba Baibulo ndi ena ochulidwa m’Malemba anali kumvelela . Lembali limatidziŵitsa za nkhani ikulu m’Baibulo yonse . Nkhaniyo ni kukweza ucifumu wa Mulungu na kuyeletsa dzina lake kupitila mu Ufumu wake . Kodi tiyenela kucita ciani kuti tipite patsogolo mwauzimu ? Komabe , kwa zaka zambili wakhala akuonekela m’mapikica a anthu ambili ojambula zithunzi . Popeza kuti Marilyn ndi James sanali kukambitsilana za mavuto ao , io anali kuuza anthu ena mmene anali kumvelela . Ndipo zimenezi zinacititsa kuti atsale pang’ono kucita cigololo . Yehova amatiphunzitsanso za colinga cake . Kukhala ndi mtima woyamikila kudzatithandiza kugonjetsa mzimu wosafuna kuyamikila ndipo tidzapilila mayeselo . Tifunika kusinkhasinkha zimene Baibulo limakamba ponena za mavuto athu . TSAMBA 28 • NYIMBO : 102 , 103 Nthawi zina mungamvele monga mmene Yobu wakale anamvelela . Komanso , nyengo inali yosiyana na ya kwathu . Baibo imati : “ Nowa anayanjidwa ndi Yehova . . . . Heidi ( Yakobo 1 : 27 ) Mulungu ni amene anayambitsa kulambila koyela kapena kuti koona . Zocita zatsiku ndi tsiku zidzakhala zosatopetsa ngati okalamba ndi owasamalila amakhala ansangala . ( Mlal . Ponena za anthu amene anali kupita ku Yerusalemu , Philo analemba kuti : “ Anthu osaŵelengeka , ocokela m’mizinda yosaŵelengeka , ena ocokela kum’maŵa , kumadzulo , kum’mwela , ndi kumpoto , anali kubwela kucikondwelelo ciliconse . Ndipo ena anali kuyenda wa pansi , kapena pa bwato . ” Na imwe mungathandizeko olo kuti nyumba yanu ni yosaukila . Popeza io adzakhala mafumu , kodi adzalamulila ndani ? Usayandikile pakhomo la nyumba yake . ” Pa Miyambo caputala 7 pali citsanzo cosonyeza kuopsa konyalanyaza malangizo amenewa . N’zoona kuti nkhawa zonse si zoipa . “ Anthu ambili amaphunzila Baibulo koma sakhala a Mboni za Yehova . ” — Denton , England . Davide anauzidwa kuti vuto limenelo lakhalapo kwa mwezi ndi masiku . Maphunzilo amenewo adzathandiza acinyamata kuikabe maganizo ao pa zinthu za kuuzimu makamaka akamakula ndi kukumana ndi zoceukitsa . — Ŵelengani Salimo 71 : 5,17 . Kodi “ cikhulupililo mwa Mulungu ” n’cofunika bwanji ? Nanga amaciyelekezela na ciani ? N’ciani cingatithandize kupewa mtima wofuna kuyanjidwa na dzikoli ? “ Mulungu wamtendele . . . ” akukonzekeletseni ndi ciliconse cabwino kuti mucite cifunilo cake . ” ​ — AHEBERI 13 : ​ 20 , 21 . Pamapeto pake , nkhaniyo inatha motele : “ Tiyeni timuitane mtsikanayo kuti timve zimene iyeyo anene . ” — Genesis 24 : 57 . Itatsegula , m’dzenjemo munatuluka utsi wambili ndipo mu utsimo munatuluka dzombe . Dzombelo silinaononge mitengo kapena zomela . Izi n’zimene zinacitikila Kalebe ndi Yoswa . Mlongo wina ku Alabama , m’dziko la United States anafunika kulimba mtima kuti adziikile zolinga zauzimu ndi kuzikwanilitsa . 4 : 2 - 8 . 24 : 45 ) Conco , pali nkhani zambili zimene mungagwilitsile nchito kuti mudye cakudya cakuuzimu . ( Aheb . 12 : 1 ) Conco , tiyeni tikhale otsimikiza mtima kugwila nchito ndi ‘ moyo wathu wonse ngati kuti tikucitila Yehova . ’ ( 2 Akorinto 9 : 15 ) Kodi mphatso imeneyi n’ciani ? Cina cimene cinanithandiza kukulitsa luso lomvela Cizungu n’cakuti n’nali kukonda kuŵelenga zofalitsa za m’Cizungu , cifukwa tinali na zofalitsa zocepa m’Citagalogi . Komabe , tikuyembekezelanso zocitika zina zosangalatsa mtsogolo . Yelekezelani kuti Mkristu wacinyamata , dzina lake Alan , akuganizila za m’bale wina wacikulile amene amavutika kuŵelenga kaamba ka vuto la maso . ( Machitidwe 24 : 15 ) Anthu “ osalungama ” ndi aja amene sanali kucita zimene Mulungu amafuna cifukwa cosadziŵa cifunilo cake . Muziyesetsa kuona zimene amacita kuti aongolele ndipo muyamikileni . Aisiraeli anaonetsa motani kuti anali anthu osakhulupilika ? Nditasiya nchito ya usilikali , koma ndisanamalize kukonza botilo , ndi pamene ndinakumana ndi Mboni za Yehova ndi kuyamba kuphunzila Baibulo . Mabanja ambili zimawavuta kucita kulambila kwa pabanja mokhazikika . Laura anati : “ Zinanditengela caka kuti ndizoloŵele umoyo watsopano . Koma tsopano sindiganizanso zobwelela kwathu ku Canada . ” Mwacitsanzo , Eli anali mkulu wa ansembe ku Isiraeli , koma ana ake aŵili aamuna anali kuphwanya malamulo a Yehova . ( Gen . 30 : 22 - 24 ) Pambuyo pake , Rakele anabeleka mwana wina wamwamuna , ndipo anamucha Benjamini . * Kupita patsogolo kwa nchito yolalikila ndi kupanga ophunzila ngakhale m’maiko mmene muli citsutso camphamvu , kwatheka cabe cifukwa ca thandizo la angelo . 4 : 19 . Blossom anati : “ Tonse anatiuza kuti tigwade . Kenako anapeleka pemphelo . Limati : “ Yehova azidzayembekezela kuti akukomeleni mtima ndipo adzanyamuka kuti akucitileni cifundo , pakuti Yehova ndi Mulungu amene amaweluza mwacilungamo . Naboti anaphedwa cifukwa cakuti anali wotsimikiza mtima kukhalabe wokhulupilika kwa Mulungu . Conco , khala wodzipeleka ndipo ulape . ” ( Genesis 11 : 31 ) N’kutheka kuti Sara anali na nchito yaikulu yosamalila kholo lokalamba limeneli . Nkhani ya pa msonkhano wacigawo m’caka cimeneco , inafotokoza kuti mipingo ya kum’maŵa kwa Ulaya ikufunika thandizo . Mabwenzi enieni ndi oona mtima kwa wina ndi mnzake , ngakhale pamene afunika kupatsa uphungu kapena kuulandila . — Miyambo 27 : 9 . 11 : 29 . Muziwasinkha - sinkha . Koma iye anaponya ‘ tumakhobili tuŵili twatung’ono ’ na mtima wonse . 3 : 18 ) Gaby anati : “ Niyamikila ngako Yehova cifukwa ca akulu acikondi amene anali nane pa nthawi yonse imene n’nali kuvutika . Ndinacita cidwi kwambili ndi cikondi ceniceni cimene cili pakati pao ndiponso mgwilizano wao . 25 : 23 . 11 , 12 . ( a ) Kodi lonjezo lofunika ngako limene munthu angapange n’liti ? Kucita kulambila kwa pabanja mlungu uliwonse kungatithandize . Nayenso Mfumu Sauli anacita mantha . Yesu anakamba kuti tiyenela kukonda Yehova ndiponso anzathu . Conco , anasiya kuseŵela chesi moimila sukulu yake . — Mateyu 6 : 33 . Padziko lonse lapansi palibe gulu limene limagwilitsila nchito kwambili dzina la Mulungu monga mmene ifeyo timacitila . ( 1 Mbiri 29 : 17 ) Pocita zopeleka zocilikizila nchito yomanga kacisi , “ anthu anasangalala cifukwa ca nsembe zaufulu zimene anapeleka , pakuti anapeleka nsembezo kwa Yehova ndi mtima wathunthu . ” Ndi umboni wina uti umene uonetsa kuti Mulungu ali ndi anthu ake ? ( Aheb . 9 : 5 ) Akelubi amenewo anapangidwa ndi golide ndipo anali okongola kwambili . — Eks . Ganizilani zocitika zotsatilazi zimene Mau a Mulungu amakamba . Amuna na akazi oopa Mulungu anali kudziŵa coyenela kucita . Mulungu amakondwela ndi cipembedzo cimene cimatsatila mfundo zoona za m’Baibulo . — Yohane 4 : 23 , 24 . M’malomwake , tizimvela malangizo ouzilidwa a wamasalimo akuti : “ Imbilani Yehova . ” Sikuti zonse zimene Ophunzila Baibo anali kucita kuyambila mu 1914 kufika mu 1919 zinali zogwilizana na Malemba . Poona malangizo onsewa a panthawi yake , kodi pangakhale cifukwa coŵelengela malangizo a m’Baibo , buku imene inalembedwa zaka pafupi - fupi 2,000 zapitazo ? ( Miyambo 25 : 15 ) Ngati timalemekeza anthu ndi kuwaganizila , cimakhala cosavuta kukamba nao mokoma mtima . Kodi wamasalimo anakamba ciani coonetsa kuti Yehova ali na mphamvu zocilitsa ? Muzipempha mzimu woyela . ( Pitani polemba kuti ZOKHUDZA IFE > ZOCITIKA ) 31 : 10 ; Zef . Tingam’fotokozele kuti ucimo wa Adamu unacititsa kuti anthu onse azibadwa ocimwa . Baibulo limasonyeza kuti ciyelo ndiponso kukhala oyela mwa kuuzimu zimagwilizana ndi kukhala waukhondo . ( Chiv . Baibulo limatilimbikitsa kutsatila mapazi a Yesu mosamala kwambili . Abale ndi alongo akaticitila zinthu zabwino ngakhale n’zocepa , zimandionetsa kuti Yehova amatikonda . ” Mwina mnzanu kapena wacibale wanu akudwala , ndipo mukudela nkhawa kuti kaya adzacila kapena ai . Iwo amayesetsa kukonza zinthu zoonongeka pa Nyumba ya Ufumu ndi kuiyeletsa . 16 , 17 . ( a ) Tingaonetse bwanji kuti timayamikila mwai wodziŵika ndi dzina la Mulungu ? ( Genesis 18 : 2 - 5 ; 19 : 1 - 3 ) Zocitika zimenezi zinalimbikitsa Akristu aciheberi kuonetsa cikondi kwa abale ao mwa kukhala oceleza . Mosiyana ndi Ahabu Mfumu yoipa , Aisiraeli ena amene anaona moto ukucokela kumwamba , anazindikila kuti Mulungu ndiye wacita zimenezo poyankha pemphelo la Eliya . Ngakhale munthu wabwino Yobu anafunsa kuti : “ Nditamuitana , kodi angandiyankhe ? ” — Yobu 9 : 16 . Kucita izi komanso kupemphela , kunamuthandiza kukhala wolimba mwauzimu . Sitifuna kuti io akhale osasangalala kapena okhumudwa cifukwa ca zocita zathu . ( Aroma 12 : 16 ) Tingamacitenso zinthu mofuna kukopela cidwi ca anthu pa ife . 28 : 13 ; Yak . 5 : 14 - 16 ) Mwacitsanzo , m’bale wina anayamba kupenyelela zamalisece ali ndi zaka 12 , ndipo anacita zimenezi mwakabisila kwa zaka zoposa 10 . Amayi na ambuya anamva cisoni kwambili . Komabe , ophunzila za mmene thupi la munthu linapangidwila apeza kuti ziwalo za thupi zimene zinali kuonedwa ngati zilibe phindu , zapezeka kuti zimagwila nchito yofunika kwambili . Koma makina osindikizila asintha kwambili pa zaka 200 zapitazi . Anali kungokamba zinthu zodzilungamitsa , ndipo anafika popempha Mulungu kuti amuuze cifukwa cake anali kuvutika . Tifunika kum’pepha mopembedzela komanso mocokela pansi pa mtima . — Afil . Yesu anafunsa ophunzila ake kuti : “ Nanga inu sindinu amtengo wapatali kuposa mbalame kodi ? ” N’cifukwa ciani macimo athu ali ngati nkhongole ? Pamene Mulungu anapulumutsa Aisiraeli mu ukapolo ku Iguputo , iye anawauza kuti : “ Ine ndine Yehova amene ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo kuti ndikusonyezeni kuti ndine Mulungu . Abale amenewa , amene ndi a “ nkhosa zina , ” amapeleka thandizo lofunikila ku Bungwe Lolamulila . Yehova akuyendatu patsogolo pako . Mtumwi Paulo anavomeleza mfundo imeneyi pamene analemba kuti : “ Pamene ndinali kamwana , ndinali kulankhula ngati kamwana , kuganiza ngati kamwana . ” ( Genesis 5 : 21 - 24 ; Aheberi 11 : 5 ; Yuda 14 , 15 ) Ngakhale n’conco , mavesi ocepa amenewo amatipatsa cithunzi cokwanila cakuti Inoki anali munthu wa cikhulupililo colimba . Mtsogolomu , pambuyo pa nkhondo ya Aramagedo , Akristu odzozedwa adzakhala mkwatibwi wa Kristu . ( Chiv . Mateyu 18 : 15 1 : 15 - 21 . Cotelo , Mulungu poyang’ana dziko lapansi anaona kuti laipa . ” Arthur anakakamizika kutuluka m’holoyo , olo kuti anadziŵa kuti sadzaloledwa kungenanso . Yesu “ anapeleka moyo wake [ na mtima wonse ] cifukwa ca ife . ” Conco tiyeni tikambilane cifukwa cake tiyenela kuona nchito yophunzitsa ena kukhala yofunika kwambili . Mutsuo anacita cidwi ngako atangoona mutu wina m’bukulo wakuti “ Zigumula za Madzi Zoopsa Kwambili Zimene Zinacitikapo . ” N’zokondweletsa kwambili kuona atsopano akupita patsogolo kuuzimu . Davide ataona zimenezi , anaipidwa kwambili . ( Eks . 7 : 1 - 3 ) Mzimu woyela unathandizanso Mose kukhala ndi makhalidwe abwino monga cikondi , kufatsa , ndi kuleza mtima . Makhalidwe amenewa anam’thandiza kutsogolela Aisiraeli . Iye anamwalila mu 2009 ndi khansa ya m’maŵele imene anavutika nayo kwa zaka 10 . Mwina munakumana ndi mavuto ambili , kapena vuto linalake limene linapangitsa kuti musinthe zinthu kwambili mu umoyo wanu . ( Mlal . YESU anali kulankhula ndi Petulo , Andireya , Yakobo , ndi Yohane , omwe anali anzake apamtima za nkhani ina yocititsa cidwi . Kupewa kupenyelela zithunzi zaciwawa sikutanthauza kuti tikunyalanyaza zinthu zenizeni . Iyai simungatelo . ( 2 Mbiri 20 : 20 - 27 ) Ici ndi citsanzo cabwino kwambili kwa ife anthu a Mulungu coonetsa zimene tiyenela kucita tikakumana ndi mavuto . Iwo anangopezako Buku Lapacaka la 2006 . Ndinapemphela kwa Yehova mocokela pansi pamtima , ndiyeno ndinaleka nchito yanga yovina . ” Mofanana ndi mlongo ameneyu , makolo ena amaona kuti ni bwino kuti mwana wawo asabatizike mwamsanga mpaka atakhwima n’kuleka kucita zinthu mwacibwana . ( Gen . 8 : 21 ; Miy . Nchito yomanga ya Yesu inaphatikizapo kumasula olambila oona ku ukapolo wa Babulo Wamkulu na kukhazikitsanso mpingo wacikhristu mu 1919 . Mwacitsanzo , iye anati : “ ‘ Mwamuna adzasiya bambo ake ndi mayi ake n’kudziphatika kwa mkazi wake , ndipo awiliwo adzakhala thupi limodzi . ’ . . . Kodi vutolo ndi laling’ono cakuti mpingo wa makolo anu ungakwanitse kulisamalila ? — Miy . Mwacitsanzo , Nehemiya anali bwanamkubwa , ndipo anafunika kusankha anthu ena a Mulungu kuti akhale oyang’anila . Kodi mtumwi Paulo anakamba kuti Akristu afunika kucita ciani ? Nanga iye anapeleka bwanji citsanzo cabwino ? ( Sal . 119 : 165 ) M’malomwake , tifunika kukhalabe okhulupilika kwa Mulungu , kupempha thandizo kwa iye , ndi kum’dalila . Kodi zizindikilo za mzimu wa kudzikuza n’ciani ? Ilaria , amene amakhala ku Italy anakamba kuti : “ Makolo anga anali kucita cidwi ndi nyimbo zimene ndinali kumvetsela . Iwo asoceletsedwa kothelatu na cikumbumtima cawo . Ngakhale n’conco , pali ena amene akalibe kufikapo kuuzimu . Akatipempha kuti tigone kumeneko , tinali kugona pansi . M’malo moona anthu kuti ndiye mmene alili , okhulupilila zakuthambo amaweluza anthu mwa kuona makhalidwe na zocita zawo . Delphine * poyamba , zonse zinali kumuyendela bwino . Kodi colinga cimeneci n’ciani ? Baibo imati “ Yehova Mulungu wathu si wopanda cilungamo , ” ndipo imatitsimikizila kuti iye sanasinthe . M’gulu la Yehova masiku ano muli abale ndi alongo amene amakonza mavidiyo , kujambula zithunzi , kuimba nyimbo , kumasulila mabuku , ndi kulemba nkhani . “ Kudzafika aneneli ambili onyenga ndipo adzasoceletsa anthu ambili . Cifukwa ca kuonjezeka kwa kusamvela malamulo , cikondi ca anthu ambili cidzazilala . ” — Mateyu 24 : 11 , 12 . Tiyenela kukhala oleza mtima . Kodi timapindula bwanji ngati tili na “ mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse ” ? Koma tifunika kuzindikila kuti Yehova ndiye mwini ulamulilo wonse . — Yes . Davide anauza Husai kuti abwelele ku Yerusalemu ndi kukadzionetsa monga bwenzi la Abisalomu , kuti akacititse Abisalomu kumvela malangizo ake osati a Ahitofeli . Malipoti aonetsanso kuti m’caka ca 1916 , anthu okwana 809,393 anapezeka pa misonkhano ya anthu onse ku America . Iwo angacite zimenezo mwa kulemba mizela iŵili , umodzi angalembe mavuto amene amapeza , ndipo wina angalembe madalitso amene amapeza . Cili monga kuti Mulungu analembelatu pa kalenda tsiku limene tidzakumana na mwana wanga m’dziko latsopano . Cigawo caciŵili cili na mabuku 27 amenenso ni “ mawu a Mulungu . ” Zinthu zocepa zimene tadzimana sitingaziyelekezele ndi cimwemwe cimene cimabwela cifukwa cotumikila Yehova nthawi zonse . ” [ 1 ] ( ndime 3 ) Abale ndi alongo ena amalephela kufika pamisonkhano pa zifukwa zina zomveka . Mwacitsanzo , pamene io anali kuphunzila cinenelo ca Cichaina , sanaike zolinga zimene sangakwanitse . Anthu amene anadzipeleka kukamenya nkhondo ndi Baraki anadzionela okha mmene Yehova anakwezela ulamulilo wake . ( Aroma 5 : 12 , 14 , 17 ) Komabe , cokondweletsa n’cakuti tili ndi ufulu wokana kulamulidwa ndi ucimo . Cifukwa Yakobo anali kufuna madalitso ocokela kwa Yehova Mulungu . 6 : 3 ) Kumbukilani malangizo a Paulo okamba za anthu oyenda mosalongosoka mumpingo . Pangano la Ufumu limapeleka mwai wotani kwa Akristu odzozedwa ? ( b ) Kodi Zion’s Watch Tower inafotokoza bwanji fanizo limeneli mu 1881 ? Iye anacita zimene mwamuna wake anakamba ndipo anati : “ Ndinadabwa mmene Mulungu anandithandizila . Nthawi zambili ndinali kungokhala cete . N’cifukwa ciani tiyenela kuyamikila cilango ca Yehova ? Mwina colinga cake cinali cakuti alepheletse kubwela kwa ‘ mbewu ya mkazi , ’ imene Mulungu analonjeza . Nanga tingaonetse bwanji kuti timam’konda ? Poyamba nchito yolalikila inali kuoneka kukhala “ yovuta kwambili ” cifukwa cakuti sinali kupita patsogolo . Zotulukapo zake , timakhala na cizoloŵezi cofufuza Mau a Mulungu tisanasankhe zocita . Kodi John anapeleka cilimbikitso cotani kwa anthu amene akulimbana ndi mavuto ? Anthu ena amati : “ Kugonana na munthu amene suli naye m’cikwati kulibe vuto . ” Mumtima mwake Gehazi anati : “ Pali Yehova Mulungu wamoyo , ndim’thamangila [ Namani ] kuti ndikatengeko zinthu zina kwa iye . ” Mulimonse mmene zinthu zilili , tiyenela kuonetsetsa kuti Nyumba yathu ya Ufumu ndi yosamalidwa bwino cifukwa cakuti imadziŵika ndi dzina la Yehova ndiponso ndi malo a kulambila koona . — Deut . N’zoona kuti kuuza ena nkhani zotelo n’kovuta . Mngelo analimbikitsa mneneli Danieli kuti : “ Udzapuma . Koma udzauka kuti ulandile gawo lako pa mapeto a masikuwo . ” Ŵelengani Machitidwe 16 : 4 , 5 . Ndipo ngati ana amakamba zabwino ponena za makolo awo , angathandize ana anzawo kuti azilemekezanso makolo awo . Akristu odzozedwa anatengela mwai nthawi imeneyi kucitila umboni . Zotulukapo n’zakuti ciŵelengelo ca Akristu odzozedwa odzalamulila ndi Kristu cinaonjezeka . Unali wakuti : “ Taonani ! Mwacitsanzo , makolo ena ku Dernmark anafanizila ndeke ndi mbalame . Rute akadzaukitsidwa , adzakondwela kudziŵa kuti mwana wake anali mbali ya mnzele wobadwila wa Mesiya . Yehova analamula Mfumu ‘ kumangilila lupanga m’ciuno mwake . ’ Pochula ena mwa anthu ake akale kuti Efuraimu , Mulungu anafunsa kuti : “ Kodi Efuraimu si mwana wanga wamtengo wapatali , kapena mwana wanga wokondedwa ? . . . Iye amatipatsa mzimu woyela moolowa manja , umene umatithandiza kukaniza maganizo oipa kuti tikhalebe oyela . * Marilyn anali kufunanso kuthandiza acibale ake ndi kusunga ndalama zodzagwilitsila nchito mtsogolo . Kodi ndi kufuna - funa zinthu zazikulu kapena kupulumuka cionongeko ca Yerusalemu monga mtumiki wokhulupilika wa Mulungu ? — Yak . Kodi mwina cingakhale cifukwa cakuti anagonjetsa Asuri kapena cifukwa Mulungu anamucilitsa mozizwitsa ? Comvetsa cisoni n’cakuti ciwembu cakeco cinathekadi . Kodi n’nakacita ciani ? Posafuna kuti munthuyo aganize kuti ndinu wamwano , mungakambe naye pang’ono ndi kuthetsa makambilanowo . 11 : 8 - 11 . ( b ) Nanga nkhani yotsatila idzayankha mafunso ofunika ati ? “ Inde Ndipita ” ( Rabeka ) , Na . Nsembe ya dipo ya Khiristu ni yofunika kwambili pa cikhulupililo cathu , komanso pa colinga ca Yehova ca poyamba cokhudza mtundu wa anthu . Kodi zimene Yesu anakamba na kucita zinali ndi zotsatilapo zabwanji ? Ena amaona kuti mau awo amamveka a cileya ndipo amaganiza kuti akamaimba , ena angaipidwe . 4 : 11 ; 21 : 3 , 4 . Ndiponso , amaikapo malipoti a mapulogalamu apadela , monga mwambo wotsiliza maphunzilo a Gileadi ndi miting’i ya pacaka . 1 , 2 . ( a ) Kodi anthu ambili amakuona bwanji kukhala munthu wauzimu ? Inu mukanakhala Yefita , kodi mukanacita ciani ? ( a ) Kodi lemba la Agalatiya 6 : 4 limatiuza kucita ciani ? N’cifukwa ciani anthu ena amalephela kuona dzanja la Mulungu pa umoyo wao ? Kodi izi si zimene kholo lililonse limafuna ? ” — Lisa . Nanga cifundo cinam’limbikitsa kucita ciani ? Nthawi zina zimenezi zingatanthauze kupatsidwa nchito zatsopano . Atamva zimenezi , amayi anakumbukila za ciphunzitso ca kuchechi kwawo , cimene cinali kunena kuti Yesu anapita ku helo , ndipo pa tsiku lacitatu anaukitsidwa . Kodi mumaganiza za abusa ataimilila kuguwa , Baibulo lili m’manja , ndipo akulalikila mokweza mau za kutha kwa dziko ? ( Yohane 8 : 32 ) Kudziŵa coonadi colongosoka copezeka m’Baibo kumatimasula ku ziphunzitso zosalemekeza Mulungu , ndi ku miyambo ya zipembedzo zambili padziko lapansi . ( Mateyu 25 : 35 - 40 ) Pa cisautso cacikulu , iwo adzaikidwa cizindikilo , kutanthauza kuti adzapulumutsidwa . Monga Paulo , ifenso tingayesetse kukhala odekha , oona mtima , ndi kukamba motsimikiza . 5 : 22 , 23 ) Eduardo anati : “ Ana athu anazoloŵela kupempha cilolezo kwa mkazi wanga akafuna kucita zinthu zina . © Paul Souders / WorldFoto [ Cithunzi papeji 6 ] Mulungu sadzalola kuti dziko lokongolali lionongedwe kothelatu M’malo mongoganizila mayankho a mafunsowo , ndi bwino kuyembekeza kuti tikaone mmene zidzakhalila . Tsiku lina n’naitana anzanga onse amene n’nali kugwila nawo nchito . Apr . 5 : 15 ) Yesu anauza otsatila ake kuti : “ Mwakutelo , onse adzadziŵa kuti ndinu ophunzila anga , ngati mukukondana . ” — Yoh . Satana anagwilitsila nchito masomphenya , koma anali kufuna kuti Yesu amugwadile zenizeni ndi kumulambila . Mmodzi wa mabwenzi a Paulo , Terofimo , anayenda naye limodzi paulendo wina waumishonale . Kucokela paciyambi pa utumiki wake , Yesu analola Malemba kum’tsogolela . ( Miy . 27 : 12 ) Koma ngati tilola anthu , ngakhale abale , kukopela zinthu za pa webusaiti yathu na kuziika pa mawebusaiti ena , kapena kuseŵenzetsa cizindikilo ca jw.org pogulitsa malonda , ndiye kuti makhoti sangatiikile kumbuyo pamene tiyesetsa kuletsa otsutsa kapena azamalonda kuseŵenzetsa molakwika zinthu zathu . 8 , 9 . ( a ) N’ciani cingatithandize kusaopa anthu ? ( b ) Tikafuna kusankha zosangulutsa , tingadziŵe bwanji zimene zimakondweletsa Yehova ? ( Gen . 12 : 5 , 10 ; 13 : 18 ; 14 : 10 - 16 ) Ngakhale n’conco , io sanaganize zobwelela ku umoyo wabwino ku Uri . — Ŵelengani Aheberi 11 : 8 - 12 , 15 . ( Yobu 14 : 13 - 15 ; Yoh . 5 : 28 , 29 ) Amuna ndi akazi okhulupilika amene anafa Khiristu akalibe kupeleka moyo wake nsembe , kuphatikizapo a “ nkhosa zina ” amene amafa ali okhulupilika kwa Yehova m’masiku otsiliza ano , adzaukitsidwa kuti apitilize kutumikila Yehova . Anthu ena akufunafuna coonadi , ndipo akucita ciliconse cimene angathe kuti acipeze . N’ciani cinawathandiza kuti akwanitse kukuka ? 103 : 20 - 22 ; Yobu 38 : 7 . Anthu amakhala “ paubwenzi ngati amakondana kwambili ndi kudziŵana bwino . ” Nayenso katswili wa mbili yakale ya Ayuda , dzina lake Flavius Josephus anakambako za kagulu kena ka Ayuda . Iye anati : “ Iwo amapewa kulumbila cifukwa amaona kuti n’koipa kwambili kuposa kunama . Iwo amakhulupilila kuti ngati munthu amacita kulumbila kuti anthu am’khulupilile , ndiye kuti ni wabodza . ” Ndipo zimenezi zimathandiza kukhala ndi makambilano ogwila mtima . Cifukwa ca ici , mlongoyu anadziŵa kuti makolo ake anali kumukonda kwambili . Ngati tiyesetsa kuphunzilapo kanthu pa zolakwa zathu , tidzakhala anzelu ndipo anthu adzatikonda . Yonatani anakhala wokhulupilika kwa Davide ngakhale kuti Yehova anasankha Davide m’malo mosankha iye kukhala mfumu yotsatila ya Aisiraeli . Mwina tingakumbukile kuti mmodzi wa mabwenziwo anali Yonatani . ( 1 Sam . Kodi umunthu watsopano umathandiza bwanji kuteteza cikwati ? Ngati banja lipanga zosankha mofulumila lingapanikizike ndipo pangakhale mikangano . ( Akol . 1 : 4 , 5 ) Ndithudi , kuganizila za madalitso amene Yehova watisungila monga atumiki ake , kumatithandiza tonse kuyang’anabe pa mphoto yathu , kaya ni yokakhala na moyo kumwamba kapena pano padziko . — 1 Akor . Mofananamo , Mulungu angatipatse “ zokhumba za mtima [ wathu ] ” panthawi yake ngati tipitilizabe kupemphela . — Salimo 37 : 4 . N’cifukwa ciani kalata ya Paulo inalimbitsa cikhulupililo ca Timoteyo ? N’cifukwa ciani Petulo analimbikitsa Akhristu anzake kuti azicelezana ? N’cifukwa ciani kampani yaona kuti ndine wosafunika pambuyo poseŵenza mwamphamvu kwa zaka zambili ? ’ Patapita zaka zingapo Yohane atalemba buku lake , zolembedwa pa zidutswazo zinagwilizana ndi zimene zili m’Baibulo masiku ano . Ndinasangalala kwambili kugwilizananso ndi banja langa . ( Sal . 36 : 9 ) Conco , ngati Mkhristu wasankha kucita zinazake kuti adziteteze iye mwini kapena kuteteza katundu wake , ayenela kuyesetsa kupewa kupha munthu kuopela kuti angakhale na mlandu wa magazi . — Deut . Koma kufunsako malingalilo a mkazi kungathandize mwamunayo kupanga cosankha coyenela . ( Miy . N’ciani cingatilepheletsa kuiona conco ? Arthur analandila kalata yomuuza kuti akaloŵe Sukulu ya Giliyadi ya miyezi 10 mu 1962 . Panthawiyo , tinafunika kupanga cosankha cacikulu . Kodi ndimadalila Yehova tsiku lililonse kuti adzasamalila zosoŵa zanga ? 16 , 17 . ( a ) Kodi anthu opulumuka Aramagedo adzakhala na umoyo wotani ? Baibulo ndi buku lapadela ndipo ndi mmene Mau a Mulungu ayenela kukhalila . Tingawathandize kuti azibwelelako kwa anthu , ngakhale amene aonetsa cidwi cocepa . ( Yeremiya 45 : 4 , 5 ) Dziko latsopano lili pafupi kwambili . Cimeneci ndico cinali cikwati coyamba . Lemba la Miyambo 25 : 11 limati : “ Mau olankhulidwa pa nthawi yoyenela ali ngati zipatso za maapozi agolide m’mbale zasiliva . ” Conco , makolo ozindikila sakakamiza ana awo kuti abatizike . Ngakhale kuti sitinakumanepo ndi Mose , Nowa ndi Yesu , kudziŵa maina ao kumatithandiza kukhulupilila kuti io anakhalakodi . Kugwila nchito mwamphamvu n’kofunika , koma sitiyenela kuiwala kuti pali zinthu zina zofunika kwambili pa umoyo kuposa nchito . Kuti tikwanilitse udindo wathu , timakhala ndi ndandanda yocita zinthu . ( Aef . 5 : 16 ; Afil . Masiku ano , pali otsalila ocepa cabe a 144,000 omwe ndi otsatila Kristu amene ndi ‘ odzozedwa ndi woyelayo , ’ Yehova . ( 1 Yoh . 2 : 20 ; Chiv . Manyuzipepala ndi wailesi zinathandiza atumiki a Mulungu kufikila anthu ambili m’malo amene munali ofalitsa ocepa Mwina inu mumaona kuti nthawi yabwino yoŵelenga Baibulo ndi m’madzulo kapena usiku musanagone . Mouzilidwa , mneneli Zekariya analemba zimene zidzacitika panthawiyo . Pali pano , ndadziŵa kuti Mboni za Yehova si Akristu ‘ a mtundu wina , ’ koma ndi Akristu oona . 119 : 66 . Tikatelo , Yesu adzatiuza kuti : “ Ndikudziŵa nchito zako , cikondi cako , cikhulupililo cako , utumiki wako , ndi kupilila kwako . Ndikudziŵanso kuti nchito zako zapanopa n’zambili kuposa zoyamba zija . ” ( Chiv . Timafunafuna anthu mu ulaliki wathu , conco timagwilitsila nchito njila zoyenela . Kodi kulalikila kungalimbitse bwanji cikhulupililo canu ? Aisiraeli okhulupilika anali kulambila Mulungu mmodzi , amene anali Mulungu wa makolo awo . Akopotala anali kuwala monga zounikila za coonadi m’dziko lonse la Japan . Kodi lembali linam’thandiza bwanji ? ( Yes . 63 : 9 ) Patapita zaka zambili , Ayuda anali ndi mantha kuti amange kacisi cifukwa adani ao anali kuwaopseza , koma Mulungu anati : “ Amene akukukhudzani , akukhudza mwana wa diso langa . ” M’nkhani yotsatila , tidzakambilana zimenezi . N’cifukwa ciani n’kofunika kuti okwatilana azizindikila mmene mnzao akumvelela ndiponso nkhani yokhudza kugonana ? * ( Genesis 37 : 4 ) Nsanje yao inali yomveka , koma kunali kupanda nzelu kulola kutengeka ndi nsanje yoipa imeneyo . Inde , umoyo wa Paulo unasumika pa zinthu za kuuzimu . Palibe amene analenga Mulungu ndipo iye alibe ciyambi . 6 : 5 , 6 ) Kuganizila mfundo imeneyi kuyenela kutilimbikitsa kupewa maganizo oipa . 27 Acicepele — Cilimikani Polimbana ndi Mdyelekezi Conco , n’zolimbikitsa kudziŵa kuti zozizwitsa za Yesu zimapeleka umboni wakuti umphawi udzatha mu Ufumu wa Mulungu . Panthawiyo aliyense adzakhala ndi cakudya cokwanila . Macmillan , tsa . 11 : 31 . Tonse tili na mwayi wothandiza pa nchito imene Yehova akucita masiku ano otsiliza . N’zacisoni kuti abale anga ena anafa cifukwa sanasinthe mtima wawo wankhanza . ( 2 Akor . 6 : 11 - 13 ) Muyenela kumvetsela mosamala kwambili wina akamakuuzani nkhawa zake . 9 : 14 , 15 ) Kwa kanthawi kocepa , “ mtima [ wa Hezekiya ] unayamba kudzikuza . ” Monga ophunzila Baibulo akhama , timayembekezela mwacidwi kudzaona amene adzakhala “ mfumu ya kumpoto ” posacedwapa . Mwamwai , mkulu wina wa mumpingo mwake anamufikila ndi kumulimbikitsa kupempha thandizo . Deuteronomo 32 : 4 Cifukwa cake n’cakuti zinthu zimene anthu amafunikila pa umoyo sizinasinthe kucokela pamene anthu analengedwa . Koma umu si mmene zinthu zinakhalila . Kodi n’zinthu ziti zimene nimaona kuti n’zopanda cilungamo ? Anakhalabe wokhulupilika ngakhale pamene ena anam’citila zinthu zoipa . Conco kukwanilitsidwa kwaciŵili kumeneku ndi kumene kuli kogwilizana ndi Ufumu wa Mulungu . Eduardo anadziŵa kuti kuti akwanitse kusamalila banja lake pambuyo pobwelela kunyumba , anafunikila kuseŵenzetsa bwino ndalama . Iye “ anangovula [ malaya ake ] n’kuwasiya m’manja mwa mkaziyo n’kuthawila panja . ” — Gen . Nditatsiliza maphunzilo , cokondweletsa n’cakuti ananditumiza kwathu ku Austria , kuti ndikapitilize kutumikila monga woyang’anila dela . 53 : 5 , 8 , 9 . Sinclair ) , Sept . Mwina mufuna kukhala mpainiya , kapena kutumikila ku magawo a cinenelo cina . Tikalandila udindo watsopano , citsanzo ca Gidiyoni ciyenela kutikumbutsa kuti sitingapambane popanda citsogozo ca Yehova ndi dalitso lake . ( Onani cithunzi - thunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) N’cifukwa ciani ana acikulile sayenela kufulumila kusiya utumiki wanthawi zonse ? Mwa ici , kulambila koona kwathandiza anthu a Mulungu kukhala ogwilizana m’mipingo na kukhala paubale wa padziko lonse . — Ŵelengani Yesaya 65 : 13 , 14 . Zimene mungacite ngati muli ndi nkhawa Tikatelo , tidzaonetsa kuti ndise “ oceleza . ” — Aroma 12 : 13 ; 1 Tim . 6 : 11 . 1 : 23 ) Lelo linonso , uthenga wabwino wokamba za cifunilo ca Mulungu ukulalikidwa pa dziko lonse . Koma iye amafuna kuti anthu asankhe ulamulilo wake cifukwa com’konda . ( b ) Ndi madalitso ati amene mufunitsitsa kudzalandila mu Ufumu wa Mulungu ? Lembali limati : “ Ndiyeno Yehova anauza Mose kuti : ‘ Uza khamulo kuti , “ Cokani kumahema a Kora , Datani ndi Abiramu ! ” ’ Anthu amenewo akuuzidwa kuti “ Bwela ! ” zakuti “ Kodi Zinangocitika Zokha ? ” Mulungu ndi “ tate wa ana amasiye ndi woweluzila akazi amasiye milandu . ” — Salimo 68 : 5 Koma kodi kucita zimenezi n’kokwanila kuti munthu akhale pa ubwenzi wabwino na Mulungu ? Tsiku lina , Jairo ali mwana , Atate anamufunsa kuti , “ Kodi pali cimene ufuna kundiuza ? ” ( 1 Yohane 4 : 10 ) Kudzela m’nsembe ya dipo ya Yesu , Mulungu anakonza zakuti tizikululukidwa macimo , tikhale ndi cikumbumtima coyela komanso ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha padziko latsopano lamtendele . Zidutswa zimenezo zili na dzina lopatulika la Mulungu lolembedwa m’Ciheberi . Ndikuika kuti uziyang’anila zinthu zambili . Otsatila a Yesu naonso anaphunzila kuti cikhulupililo n’cofunika pokhululukila ena Mwacitsanzo , m’caka ca utumiki ca 2014 , anthu oposa 275,500 anabatizidwa kukhala Mboni . Popeza kuti kupilila kumatithandiza kukhala Akristu ofikapo , sitiyenela kuphwanya malamulo a Yehova kuti tithetse mavuto . Mogwilizana ndi Genesis 41 : 42 , tiphunzilapo ciani pa zimene zinacitikila Yosefe ? 3 Mbili Yanga — Poyamba N’nali Wosauka , Koma Lomba N’nalemela Anthu anali kucitabe cinyengo ndi zinthu zina zoipa , ndipo nchito yomanga kacisi wa Yehova ku Yerusalemu inali kutali kuti isile . Kodi tingasonyeze kuti timalemekeza Yehova ngati timaphonya misonkhano popanda zifukwa zomveka ? Zimenezi zinatithandiza kuzoloŵela kwambili cinenelo ndi umoyo wa kumudzi . Ico cimakhulupilila zinthu zonse zimene Mulungu anakamba m’Mau ake a coonadi . — 1 Akor . Imafotokozanso mavuto amene amatulukapo cifukwa ca kusadziletsa . Yehova walola “ olamulila akuluakulu ” amenewa kutilamulila , ndipo amafuna kuti tiziwalemekeza . ( Mat . 6 : 10 ) Pamene tiyembekezela mapeto a dzikoli amene akuoneka ngati akucedwa , ena angafunse kuti , ‘ Kodi tifunika kuyembekezelabe ? ’ Kuwonjezela apo , Mdyelekezi amacita ciliconse cotheka kuti aiwalitse anthu ambili dzina la Mulungu . Anapempha kuti wina adzakhale kudzanja lake lamanja , wina ku lamanzele . — Maliko 10 : 35 - 40 . Mame amadontha pang’onopang’ono . Tisaleke kumuyamikila Yehova potikokela kwa iye kupitila mwa Mwana wake , “ Mtumiki Wamkulu ndi Wokwanilitsa cikhulupililo cathu . ” Kumene malamulo salola munthu kukhala na mfuti , kapena kumene kuli malamulo a kasewenzetsedwe ka mfuti , Akhristu ayenela kutsatila malamulowo . — Aroma 13 : 1 . Kodi Akristu okhulupilika masiku ano adzakhala ndi mwai wotani mtsogolo ? Masiku ano , pali zinthu zambili zimene zingatisokoneze potumikila Yehova kuposa mmene zinalili m’nthawi za m’Baibulo . Timayamikila ngako zimene iwo amacita potithandiza kuonetsa cifundo na cilungamo kwa wina na mnzake mumpingo . M’malomwake , anasankha kumvela aneneli a Yehova monga Yesaya , Mika , ndi Hoseya . Koma ndimakwanitsa kucita zofunika za tsiku ndi tsiku ndili ndi nkhawa zocepa cifukwa ca pemphelo . Jerome anakonza zambili mwa zolakwika zimenezi . ( Eks . 34 : 6 ) Pamene tiyesetsa kutengela khalidwe la Mulungu losakwiya msanga ndi kufatsa , timaonetsa nzelu , ndipo Yehova amakondwela kwambili . — Aef . Kodi “ paladaiso ” amene Paulo anaona amatanthauza zinthu zitatu ziti ? Koma cisoni n’cosiyana kwambili ndi zimenezi . Iye anaphasa bwino ku sukulu , ndipo anali na colinga cocita maphunzilo apamwamba . Cingalawa cinali umboni wakuti Nowa anali na cikhulupililo . Nawonso ubatizo wocitidwa pamaso pa anthu umacitila umboni za wobatizikayo . Kenako , m’pempheni kuti mukabwelenso kudzakambilana zoonjezeleka ponena za Yehova Mulungu . Iye anali kulalikila kwa osauka na olemela , kwa Afarisi na Asamariya , ngakhalenso kwa okhometsa msonkho na ocimwa . Kudzicepetsa n’kofunika kuti ‘ tizimvela amene akutsogolela ’ mumpingo ndi kutsatila malangizo amene gulu la Yehova limapeleka . — Aheb . Pamene iye anali kukalamba , akazi ake anali “ atapotoza mtima wake moti iye anali kutsatila milungu ina . . . Cotelo Solomo anayamba kucita zinthu zimene zinali zoipa m’maso mwa Yehova . ” ( 1 Maf . Nili ku sekondale , n’nali na mnzanga amene anali katswili wa nkhonya . Muyenela kuti mukumbukila bwino mmene munamvelela mutazindikila kuti mwapeza golide wa kuuzimu . Kuŵelenga Baibulo mokweza kudzakuthandizani kumvetsetsa ndi kukumbukila kwambili zimene mwaŵelengazo . Nayenso Satana sacita cifundo ndi anthu amene amafuna kuwagwila . Imeneyi ndi mphatso yocokela kwa Mulungu . ” Iye amaonanso kuti timamukonda kwambili , ndiponso timafuna kum’tumikila ndi mtima wonse . Iwo anali kuyesetsa kuniphunzitsa monifika pamtima . Pamene matenda anakula , ndinamufunsa kuti , “ Kodi unaonapo munthu ali kufa ? ” Mungacite ciani kuti mukhalebe maso mwauzimu ? 11 : 28 - 30 . Tsankhu ndi kupanda cilungamo n’zofala kwambili . CINTHU cimodzi cimene cimasiyanitsa anthu na nyama n’cakuti anthu analengedwa na cikumbumtima . ( Chivumbulutso 19 : 11 - 21 ) Ngakhale kuti mau ambili a lemba limeneli ndi ophiphilitsa , tinganene kuti Mulungu adzagwilitsila nchito makamu a angelo kuononga adani ake . Cofunika kwambili ndico kusinkha - sinkha ndi kuyesetsa kucita zimene mwaŵelenga . Tiyamikila kwambili nsembe ya Khiristu , cifukwa imatimasula mu ukapolo wa dzikoli lolamulidwa ndi Satana , ndipo sitiopanso imfa . — Aheb . ( Romans 15 : 26 ) Mofananamo , timathandiza amene akhudzidwa ndi ngozi za cilengedwe mwa kuwamangilanso nyumba zao , Nyumba zolambilila ndi kuwapatsa zakudya , zovala , ndi thandizo la mankhwala . Pankhani imeneyi , mtumwi Paulo anakamba kuti : ‘ Ucimo unaloŵa m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi , ndi imfa kudzela mwa ucimo , imfayo n’kufalikila kwa anthu onse cifukwa onse anacimwa . ’ ( Yakobo 4 : 8 ) Ndiyeno cikhulupililo cathu mwa Yehova cidzalimba kwambili . Kodi mumakhalabe okhulupilika kwa Yehova , kapena mumacita zinthu zomwe anzanu amacita kuti asakusekeni ? Komabe , omasulila ambili salemba dzina la Mulungu m’Mabaibulo ao . Cifukwa ca nchito yolalikila ndi kuphunzitsa imene Mboni za Yehova zimagwila padziko lonse , anthu ambili aphunzila kulambila Mulungu motsogoleledwa “ ndi mzimu ndi coonadi . ” Kucita zimenezi kudzatilimbikitsa kutengela kwambili makhalidwe ake . Ndiyeno , anaganiza zouza a Doris kuti adzawapezela wina wowaphunzitsa . Pa mphatso zonse zabwino zimene Mulungu anapatsa anthu , n’cifukwa ciani dipo ni yamtengo wapatali ? Mwacitsanzo , pa Oweruza 5 : 20 , 21 pamati : “ Nyenyezi zinamenya nkhondo zili kumwamba , zinamenyana ndi Sisera zili m’njila zawo . Yelekezelani kuti muli m’dziko la tsopano . Zinthu zonse zimene Yehova analosela ponena za masiku otsiliza zakwanilitsidwa . Kodi tingapilile bwanji cisoni ? Mwacitsanzo , mabungwe ena amaopseza abale kuti adzawacotsa m’dzikolo kapena adzaleka kuwathandiza ngati akana kugwila nchito imene imacititsa kuti aziphonya misonkhano . Mwacitanzo , mukhoza kukhala na zolinga monga izi : ‘ Nifuna kudziŵa zambili ponena za Mulungu . ’ Kukonda Mulungu kumatanthauzanji ? Panthawi ina , Baruki mlembi wa Yeremiya , anali kufuna kukhala ndi zinthu zazikulu . Izi zinam’cititsa kuti asamasangalale potumikila Mulungu . Na imwe mufunika kupitiliza kunola luso lanu . Ndiyeno padzafika nthawi ya masautso [ cisautso cacikulu ] imene sinakhalepo kuyambila pamene mtundu woyambilila wa anthu unakhalapo kufikila nthawi imeneyo . ( Levitiko 12 : 3 ) Capezeka kuti magazi a makanda amatha kuundana mosavuta pakapita wiki imodzi kucokela pamene anabadwa . 11 : 23 - 25 ) Mkate umaimila thupi la Yesu langwilo limene linapelekedwa monga nsembe , ndipo vinyo amaimila magazi ake amene anakhetsedwa . MBILI YANGA : NDINALI WACINYENGO NDI WANJUNGA ( b ) Kodi inu mumakonda kwambili vesi iti m’Malemba a Ciheberi ? Luca sanangofotokoza zimene amakhulupilila , koma anaonetsanso anzake onse a m’kilasi webusaiti yathu . Colinga cathu cimakhala cakuti tilimbikitsane ndi abale athu , osati kuti tidzionetsele ndi zimene tili nazo . 4 : 25 ) Koma nthawi zina , kucita zimenezi kungakhale kovuta . N’ciani cimacititsa gulu lathu la abale padziko lonse kukhala locititsa cidwi ? Jowana anali mmodzi wa akazi ambili amene Yesu anacilitsa . Kodi malonjezo a Mulungu tingayambe kuwaona bwanji kusiyana ndi mmene tinali kuwaonela kale ? Kuti mukhale ndi cithunzi ca Ufumu wa Mulungu m’maganizo mwanu , ‘ yang’anitsitsani , ’ kapena ganizilani mmene umoyo wanu udzakhalila m’Paladaiso . Koma limatanthauzanso zimene iye amacita zokhudza nchito imene Mboni zake zimacita kuti akwanilitse cifunilo cake . Pamene mukudzipeleka kwa Yehova , mumamuuza kuti tsopano ndinu ake . Nkhani ya “ Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi , ” imene inafalitsidwa mu Nsanja ya Mlonda ya July 2016 , inakamba kuti : “ Kupitila mwa mneneli wake Ezekieli , Yehova analosela kuti anthu [ ake ] adzabwelela ku Dziko Lolonjezedwa ndi kugwilizananso kuti akhale mtundu umodzi . 3 : 11 , 12 ) Yehova amakumbukila olungama ndipo amawadalitsa . Ngati ana anu amvela Mau a Mulungu ndi kutengela citsanzo canu cabwino , mudzamvela monga mmene Yohane anamvelela atamva za ana ake auzimu . 105 : 17 , 18 ) Ngakhale kuti Yosefe anacita zinthu zacilungamo , anaoneka monga akulangidwa m’malo modalitsidwa . Makolo amene ali na nzelu zopindulitsa amaganizila mmene angalangile ana awo , komanso mmene cilangoco cingakhudzile anawo mtsogolo . Kuti mudziŵe zosoŵa za munthu amene mufuna kupatsa mphatso , funsani ena amene analiko m’cocitika cofananaco . Koma anapitilizabe kukhala mbali ya mpingo . Pa cifukwa cimeneci , Yehova anam’kana kuti asakhalenso mfumu ya Aisiraeli . Popeza n’zosatheka kulimbitsa cikhulupililo mwa mphamvu zathu , tifunika kupempha Mulungu kuti atipatse mzimu wake woyela . Ngati mfundo yakuti anthu abwino sadzakumananso ndi mavuto yakukondweletsani , bwanji osayamba kuphunzila Baibulo kuti mudziŵe za Mulungu woona ndi cifuno cake ? Kodi mudziŵa zimene Baibo ikamba pankhani ya masiku akubadwa ? Ni buku lakale kwambili kuposa ena oculuka . Pamene Petulo anali kupeleka cenjezo lakuti sitifunika kuseŵenzetsa ufulu wathu molakwika , anakambanso njila yabwino yoseŵenzetsela ufuluwu . Conco tiyeni tiwafunse . Amafunanso kukhala ndi mabanja abwino , na mabwenzi abwino . Conco , Mkristu wodzozedwa ayenela ‘ kudzifufuza ’ asanadye zizindikilo zimenezo . Mu mpingo wacikhristu masiku ano , muli ena amene poyamba anali “ okonda kukwiya , ” koma manje ni oganizila ena , okoma mtima , oleza mtima , ndipo amacita zinthu mwamtendele na ena . * ( Miy . Mulungu anatumiza mngelo kukam’limbikitsa . Makolo athu anali kugwila nchito mwakhama . Mu 1925 , makolo anga anakumana ndi a John Papparizos , amene anali Wophunzila Baibo wakhama ndi wansangala . Yesu anakamba fanizo la mkazi wa masiye wosauka amene anali kupita kwa woweluza wosalungama kukapempha thandizo . Ni mau ati amene akutipatsa cithunzi ca nthawi ya ciukililo copita kumwamba ? Iye anacita pangano ndi Davide pamene anali Mfumu ku Yerusalemu . Ndipo anam’lonjeza kuti Mesiya adzacokela m’banja lake . Ndipo tifunikanso kutsatila ziphunzitso zonse zacikritsu paumoyo wathu . Kodi mwaona cifukwa cake zimenezi n’zolimbikitsa kwa ife ? ( Yakobo 3 : 17 ) Conco , Baibulo limaphunzitsa kuti tiyenela kupewa zosangulutsa zilizonse zimene zingaticititse kuganizila kapena kulakalaka zinthu zoipa . Izi ziphatikizapo kuwaphunzitsa mavalidwe okondweletsa Mulungu . Patapita zaka 25 , a David anabwelela kwa Yehova , ndipo io ndi akazi ao tsopano akutumikilanso Yehova pamodzi mosangalala . Nikapemphela , mzimu wake umanipatsa mphamvu . Njila yaciŵili , kuganizila cikondi ca Yehova kudzatithandiza kukhala odzicepetsa . “ Yehova anayala maziko a dziko lapansi mwanzelu . ( Numeri 25 : 3 ) Aisiraeli anafunika kumakumbukila kuti Mulungu wawo , “ Mulungu woona , ” ni wapadela . Nakhala na Mwayi Wotumikila Pamodzi ndi Amuna Auzimu ( D . Yesu anauza ophunzila ake kuti ‘ apite ’ kwa anthu onse . ( Miy . 27 : 23 ) Kuti mucite zimenezi , muyenela kudziŵa zocita za ana anu , zimene amaganiza , ndi zimene amafuna . Akhristu ambili acicepele sanapusitsike na cinyengo ca Satana cimeneci . Mmodzi wa iwo ni mlongo Kiana , wa zaka 20 . Ndipo walonjeza kuti adzatifupa cifukwa ca kukoma mtima kwathu . N’cifukwa ciani anthu amafa ? Timakonda kuphunzitsako ena za Yehova ( a ) Ndi udindo wotani umene Mulungu anapatsa Adamu ? 3 : 5 , 6 ) Kodi n’zoona kuti Mulungu amathandiza ? Pambuyo pakuti mwininyumba waŵelenga kapepalako , tinali kumugaŵila kapepalako ndi kupitiliza ulendo . ” Tsiku lina , zaka zoposa 3,000 zapitazo , Yehova anauza mneneli Samueli amene anali wokalamba panthawiyo kuti : “ Maŵa nthawi ngati ino ndikutumizila munthu kucokela ku dela la Benjamini , ndipo udzam’dzoze kukhala mtsogoleli wa anthu anga Isiraeli . ” ( 1 Sam . Kuti titeteze ubwenzi wathu ndi Yehova , tiyenela kucitapo kanthu mwamsanga ndi mosazengeleza . Daniel anadziŵa kuti zimenezi zinali zoona , cifukwa mkazi wake Miriam anali atayamba kale kucita upainiya , ndipo anali kukhala wosangalala . Kodi mukukwanilitsa malonjezo anu kwa Yehova ? Iwo adzasoŵa kothawila . Ngati Watchtower Laibulale kapena Laibulale ya pa Intaneti ilipo m’cinenelo cake , mungamuonetse mmene angaiseŵenzetsele pofufuza mayankho a m’Baibulo . Mu 1983 , nthambi ya ku Australia inayamba kusindikiza Nsanja ya Olonda ya masamba 24 kamodzi pakapita miyezi itatu . Yesu anali kudziŵa bwino kuti m’dongosolo loipali , padzakhala zinthu zambili zotangwanitsa ndi zodetsa nkhawa . Iye anatsindika mfundo yakuti io ayenela kukhala okhulupilika ndiponso kuthandiza abale a Yesu odzozedwa padziko lapansi . 3 “ Ndidziŵa Kuti Adzauka ” Pa zaka 70 zotsatilapo , ndinaganiza zocita monga mmene Paulo analangizila Timoteo kuti , “ lalikila mau . Lalikila modzipeleka , m’nthawi yabwino ndi m’nthawi yovuta . ” — 2 Tim . Mwa kukamba mau akuti “ ticite , ” mwacionekele Mose anali kutanthauza kuti wotulutsa madzi adzakhala iye na Aroni . 22 : 35 - 40 ) M’cikondi muli makhalidwe ambili a Cikhiristu , kuphatikizapo cikhulupililo . Iye anauza ophunzila ake kuika maganizo ao pa nchito yolalikila imene anali kugwila . Mkuluyo anakambanso kuti : “ Tsiku lina , Graham ananiuza mau ocititsa cidwi . Mwamunayo analandila thandizo lake . Taylene , amene tamuchula poyamba paja , anati : “ Munthu angauze Mulungu ciliconse cimene akufuna . ” Mwa ici , madalitso onse ochulidwa m’mavesi 12 mpaka 14 anali kumveka kuti ni opita kwa anthu oipa , amene achulidwa m’mavesi am’mbuyo . M’bale Ramu anakamba nkhani yake yoyamba m’sukulu ya ulaliki mu 1944 . Monga Akhristu odzipeleka , tinadzikana tekha ndipo tinasankha kukhala na umoyo wotsatila ziphunzitso za Khristu monga ophunzila ake . “ Ine Ndinauka Monga Mai mu Isiraeli ” 12 Paulo anacita khama kuphunzitsa Timoteyo ‘ mmene amacitila zinthu potumikila Khiristu . ’ ( Genesis 2 : 10 - 14 ) Mitsinje iŵili imeneyi imathila madzi m’Nyanja ya Perisiya , kupitila m’dziko limene tsopano ni Iraq , dela la Perisiya wakale . Tikhoza kupitiliza kum’tumikila mokhulupilika ngakhale ndife ofalitsa cabe . Imwe acicepele , kodi n’ciani cingakuthandizeni kupanga zosankha mwanzelu ? Kungokwela basi iliyonse imene mwakonda kungacititse kuti musocele . Anthu olimbika amapewanso kugwila nchito mopitilila malile . N’cifukwa ciani gulu la Yehova likukulilakulila ? 4 : 7 ) Tifunika kukhala na maganizo monga a mtumwi Paulo . Tidzayamba kukamba nawo pa nthawi yoyenela za kufunika kodzipeleka na kubatizika . Mulimonse mmene zingakhalile , sitiyenela kuwakakamiza kuphunzila coonadi . M’nkhani yaciŵili , tidzaona njila zosiyana - siyana zimene tingaonetsele kuti timayamikila mwayi wokhala anthu a Yehova . Ndiponso salola citsutso kuwacititsa kuleka kutumikila Mulungu woona . Apanso , Yehova analonjeza bwenzi lake Abulahamu kuti adzam’culukitsila mbeu yake . Timaonetsa nzelu mwa kupewa anthu amene ali na makhalidwe ochulidwa pa 2 Timoteyo 3 : 2 - 5 . Malo athu olambilila amenewa ndi mphatso yamtengo wapatali ndiponso cuma capadela cimene Yehova watipatsa . Onelelani vidiyo yakuti Philippines Typhoon — Faith Conquers Adversity pa www.jw.org . Nabwela kuno cifukwa akulu akonza zimenezi . Tsiku lotsatila , mkazi wa mwamuna amene anataya ndalamayo anapita ku nyumba ya Haykanush kuti akawathokoze pa zimene anacita . Iye anawacondelela kuti atenge ling’i ya dayamondi . ( Ŵelengani Machitidwe 10 : 28 , 34 , 35 . ) Nayenso Antonio anati : “ N’nali kuceza naye kaŵili - kaŵili Federico . Katswili wina anafotokoza mmene munthu wonyada kwambili amadzionela . Analemba kuti : “ Mu mtima mwake amakhala ngati ali na kaguwa , kamene amapitapo kukagwada n’kumadzilambila . ” Kodi anthu ena tingawaceleze m’njila ziti ? Kodi mfundo imeneyi igwilizana bwanji na nchito yathu yolalikila ? ( b ) Nanga fanizoli timalimva bwanji masiku ano ? Koma nthawi zina makolo amafunikila kulanga ana , kumene kuli ngati kudulila maluŵa . Ganizilani cabe , n’nafunika kuseŵenzetsa mendo pogwila foloko na spuni kuti nidye . Patapita nthawi , tinakhala wokonzeka kubala zipatso . ▪ Anthu a Yehova “ Aleke Kucita Zosalungama ” Miyambo 4 : 13 imati : “ Gwila malangizo , usawataye . ( Miy . 15 : 23 , 30 ) Kuwonjezela apo , kuŵelenga Nsanja ya Mlonda kapena zofalitsa za pa webusaiti yathu kungalimbikitse munthu wopanikizika m’maganizo . Tsiku lina pamene ndinali kuyenda pamseu , belo locenjeza linalilanso . 20 , 21 . ( a ) Kodi mphunzitsi wabwino amacita ciani ? Iye akuuzani kuti , “ Iyayi , ici calimbana na mphepo na mvula za mphamvu . Iyi ni njila ina imene Atate wathu wacikondi , kupitila m’Mau ake , amathandizila ndi kutonthoza anthu amene akumana ndi mavuto aconco . M’kalata yoyamba youzilidwa imene Paulo analembela Akhristu odzozedwa a ku Akorinto , iye anakamba kuti mwa kucita Cikumbutso ca imfa ya Yesu caka ciliconse , iwo ‘ amalengezabe imfa ya Ambuye mpaka iye adzafike . ’ ( 1 Akor . Ngakhale n’conco , Davide anali kudziŵika kuti ndi mwamuna wankhondo wolimba mtima ndipo ayenela kuti anali ndi zaka pafupifupi 20 panthawiyo . — 1 Samueli 16 : 18 ; 17 : 33 . Ganizilani izi : Mumaonetsetsa kuti ana anu apita kusukulu cifukwa mumadziŵa kuti maphunzilo ndi ofunika kwambili , ndipo mumafuna kuti azisangalala kuphunzila zinthu zatsopano . Kodi Mkhristu ayenela kucita ciani zinthu zikakhala conco ? Kodi zofunika kwambili kwa inu ndi ziti ? Poganiza kuti adzapambana , Kolosase anayenda kukacita nkhondo na Koresi , koma “ ufumu wamphamvu ” umene unagonjetsedwa unali wake ! 5 : 25 ; Aheb . Kuseŵenzetsa mfundo za m’Baibo kungathandize banja kukhala lamtendele ndi lacimwemwe , ndipo kungathandizenso kuti banjalo likalandile mphoto . Ndipo izi ziyenela kuti zinalimbitsa kwambili cikondi cawo kwa Paulo komanso pakati pawo . Akaona zimene acita , amawadalitsa mogwilizana ndi nchito zawozo . Ndiye cifukwa cake sitiyenela kuweluza anthu a m’gawo lathu kapena a mumpingo mwathu . Akristu odzozedwa mphoto yao ndi moyo wosafa kumwamba , ndipo adzalamulila pamodzi ndi Yesu monga mafumu . 9 Mtendele — Kodi Mungaupeze Bwanji ? Coyamba , io anali kufunsa ngati sanamvetsetse , ndipo anali kucita khama kuti azindikile tanthauzo la zimene Yesu anali kukamba . ( Mat . Sembe kuti timacita zonse zimene Yehova amafuna popanda kulakwitsa ciliconse , kukoma mtima kwake kukanatiyenelela . Tingaonetse bwanji kuti timayamikila mwayi wodziŵa coonadi ? Zimene zinacitika n’zakuti mwana wake mmodzi yekha , amene anali wamkazi , ndiye anatuluka kukamucingamila atapambana nkhondo . Usiku umodzi cabe , “ mngelo wa Yehova anapita kumsasa wa Asuri n’kukapha asilikali 185,000 . ” — 2 Maf . Malambawo anali kukhalanso na tuzitsulo tolimba tokoloŵekapo lupanga na mpeni . Ngati abululu athu amatitsutsa cifukwa colambila Yehova , tifunika kupitiliza kuwakonda . M’bale wina anatipatsa malo ogona tonse , kuphatikizapo m’bale Pryce Hughes , amene panthawiyo anali mtumiki wa nthambi ku Britain . N’zolimbikitsa ngako kuti Akhristu ambili azindikila kuti nchito imeneyi ifunika kugwilidwa mwacangu , cakuti ena akukhala na umoyo wosalila zambili pofuna kuwonjezela zocita mu ulaliki . Mobweleza - bweleza Davide ayenela kuti anali kuwamvela akuchula dzina la munthu wina - wake amene anali kumuopa . Conco , tifunika kumasinkha - sinkha zimene taŵelenga . Timadziŵa bwanji kuti timabalabe zipatso ngakhale ngati tikulalikila m’gawo louma ? 15 : 19 , 25 ) Yesu anamva kuti m’thupi mwake mwatuluka mphamvu . Conco anafunsa kuti adziŵe amene anamugwila . Atate anali mtumiki wa mpingo ( dzina lakale la mgwilizanitsi ) . Anthu amenewa ndi andale , apolisi , akuluakulu a boma , opanga malamulo , ndi oweluza . M’bale Harry Peterson ndi amene anali kutiphikila . Zinali zosavuta kwa ife kumuchula ndi dzina lake lotsiliza lakuti Peterson m’malo mochula dzina lake leni - leni , lakuti Papargyropoulos . Mukacita zimenezi , mudzasunga nzelu zopindulitsa , ndipo mudzapeza moyo wosatha . — Miy . Bwanji ponena za cifukwa cimene anthu adzaweluzidwila kuti ndi nkhosa kapena mbuzi ? Takambilana makhalidwe angapo oipa amene Akhristu afunika kuleka kapena kuwapewa . Yesu ndi ophunzila ake sanatsatile miyambo imeneyi , m’malo mwake iye analola Jowana ndi akazi ena okhulupilila kuti aziyendela nao limodzi . Koma iye sakuwamvela . Apitiliza kuseŵela na bolayo , ndipo akuphwanya mphika wa maluŵa . Iwo anali kufunafuna anthu amene anali kufuna kudziŵa coonadi . Pamene mkulu anali kukamba Fernando anamvetsela . Barry , amene analelapo ana anai anati : “ Kuuza ana cifukwa cimene mwacitila cinthu cina cake kumawacititsa kukukhulupililani . ” Nikolai anatifotokozela zimene zinacitika . Iye samakuuzani kuti muyenela kuthela nthawi yanu yonse kulalikila za Ufumu . Anali kupaka ngalawa zao ndi phula limeneli . Phula lamadzimadzi linali kuuma ndi kulimba cakuti linali kupanga muyalo umene unali kuteteza kuti madzi asaziloŵa m’ngalawa . Mwacitsanzo , ena a ife mwina timakonda kuŵelenga mabuku , kuonelela TV , kukaona malo osangalatsa , kugula zinthu , ndi kufufuza zipangizo zatsopano kapena zinthu zapamwamba . Iwo anamva kuti anzao ambili a kusukulu anasangalala kwambili atapenyelela vidiyo imeneyo . Ndi liti pamene ‘ imfa , mdani wotsilizila , idzaonongedwa ’ ? N’cifukwa ciani tinganene kuti Yehova ndi Mpatsi Wamkulu ? 7 , 8 . ( a ) Kodi kudziikila zolinga kumathandiza bwanji munthu kupanga zosankha mosavuta ? Kuti timvetsetse mfundo imeneyi , tiyeni tiyankhe mafunso anai ofunika kwambili . Anali kudziona monga olimba kwambili m’coonadi cakuti sangagwe mwauzimu . ( 1 Akor . Kodi zizindikilo zodabwitsa zimenezi tidzaziona ndi maso pamene ulosi umenewu udzakwanilitsidwa ? N’nafika pokhala katswili m’maseŵela amenewa . Cifukwa mau a Mariya ndi ofanana ndi mau amene Hana , mai wa Samueli , anakamba m’pemphelo lake . Kubatizika kumatipatsa mwayi wolandila madalitso ambili , koma kumabweletsanso udindo . Pamene Manowa anauzidwa uthengawo ndi mkazi wake , iye anakondwela kwambili . Komabe , anthu ambili amaona kuti cimene cinayambitsa umbeta wacipembedzo ni ciwelewele cimene cafala pakati pa abusa a zipembedzo zosiyana - siyana . Kumbukilani kuti kudziŵa Malemba ndiwo maziko a ubwenzi wolimba na Yehova . 9 : 34 ) Popanda thandizo la Yehova , sitingapambane pa nkhondo yathu yolimbana ndi Satana . Anthu ambili onyada amaganiza kuti kudzicepetsa ndi kukhala wopola kapena wodzikaikila . Pali “ kupembedza koyela ndi kosaipitsidwa kwa Mulungu ndi Atate wathu . ” ( Aef . 4 : 11 , 15 ) M’malo modzicha dzina lapamwamba lakuti mtumwi , “ ophunzilawo anayamba kuchedwa Akhiristu , motsogoleledwa ndi Mulungu . ” Yehova Mulungu ni citsanzo cabwino kwambili pankhani yoonetsa kufatsa ndi kuleza mtima . ( Ŵelengani Deuteronomo 3 : 28 . ) Pang’ono ndi pang’ono nkhawa zanga zinayamba kucepa . ( Aroma 6 : 12 ) ‘ Tingalole kuti ucimo uzilamulilabe ’ ngati timangocita zinthu malinga ndi zilako - lako za thupi lathu locimwa . Ndipo anaonjezelanso kuti : “ N’zoona kuti munthu akakhumudwa amalankhula mosasamala , koma si bwino kulankhula mozazuka . ( Ekisodo 3 : 7 , 8 ) Caka ndi caka , Ayuda kulikonse amacita cikondwelelo ca Pasika kuti akumbukile kumasulidwa kwawo . — Ekisodo 12 : 14 . Amakhumudwa mwamsanga , kukhala na nkhawa , komanso kuvutika maganizo maningi M’Baibulo la American Standard Version lotulutsidwa mu 1901 munali dzina la Mulungu , koma limene linatulutsidwa mu 1952 munalibe dzina la Mulungu . Ngati muli na pulogilamu ya JW Language m’cinenelo canu , ingakuthandizeni kudziŵa mmene mungapatsile moni anthu ocokela ku maiko ena m’cinenelo cawo . — Ŵelengani Afilipi 2 : 3 , 4 . Mose anali kuganizila kwambili za Yehova ndi anthu ake . Yesu ataukitsidwa , anauza khamu la otsatila ake kuti : “ Pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzila anga , muziwabatiza . . . , ndi kuwaphunzitsa kusunga zinthu zonse zimene ndinakulamulilani . ” Malinga ndi kuona kwa munthu , Mose sanali kanthu kwa Farao . 2 : 23 . Mofanana ndi mmene zinalili ndi Cigiriki , anthu ambili amakamba Cingelezi masiku ano makamaka pankhani zokhudza malonda ndi maphunzilo . Koma zikutanthauza kuti tiyenela kukonda kwambili Yehova kuposa wina aliyense . Yesu anacenjeza otsatila ake kuti : “ Kapolo sangatumikile ambuye aŵili , pakuti adzadana ndi mmodzi ndi kukonda winayo , kapena adzakhulupilika kwa mmodzi ndi kunyoza winayo . Koma ciŵeluzo ca dzikoli cinapelekedwa ndi Wolamulila wa cilengedwe conse , amene ndi wangwilo komanso wacilungamo . Tiyenela kukhala monga Yakobo , amene sanafooke polimbana ndi mngelo mpaka atam’dalitsa . Molingana ndi zimene zinacitikila Solomo , vuto limodzi lalikulu limene lingaike umoyo wathu wauzimu paciopsezo ni kukhala pa ubwenzi ndi anthu amene sadziŵa kapena kulemekeza miyezo ya Yehova . Tiyenela kucitapo kanthu kuti tithandize ena , ndipo tikacita zimenezo tidzakhala odekha ndi acikondi . Abale amenewa ndi odzipeleka kucita utumiki ulionse umene apatsidwa . 9 : 11 , 12 , 24 ) Malinga n’zimene Yesu anakamba , iye “ sanabwele kudzatumikilidwa koma kudzatumikila ndi kudzapeleka moyo wake dipo kuombola anthu ambili . ” ( Mat . ( Yobu 26 : 14 ) Ngakhale n’conco , zocepa zimene timadziŵako za mapulaneti , nyenyezi , na milalang’amba , zimatipangitsa kuvomeleza kuti zinthu zakuthambo zinalinganizidwa mwa dongosolo lodabwitsa . ( Sal . N’ciani cimene akulu ku Isiraeli anali kucita pofuna kuonetsa cilungamo ca Yehova ? N’cifukwa ciani tikunena telo ? Palibe Mkristu amene mwadala angafune kuti mnzake azilephela kupezeka pa misonkhano yacikristu . M’bale Hughes anati : “ Tifuna anthu amene ali na mamotoka kuti akagwile nchito yapadela yogaŵila tumabuku tumenetu m’dzikolo . ” Atamvetsa coonadi , analeka kumenya nkhondo . Komabe , zinthu zimenezi zacititsanso mavuto ena . Mwacitsanzo , ganizilani za Baibo yomasulidwa m’Cizungu ya King James Version . Gidiyoni anakonza cakudya ndi kupatsa mngeloyo . 11 : 24 - 26 ) Tiyeni titengele cikhulupililo ca atumiki amakedzana amenewa , cocengeta bwino mphatso yathu ya ufulu wosankha zocita , poigwilitsila nchito kucita cifunilo ca Mulungu . Ŵelengani Salimo 97 : 10 . Buku la Mateyu limafotokoza kwambili zokhudza Yosefe . Mwacitsanzo , limakamba zimene iye anacita atadziŵa kuti Mariya ali na pakati . Poyamba ndinali kukhala pakhomo pao . Muyenela kuuza ana anu kuti kuonelela zamalisece n’koipa . Koma anali kujambula Yesu malinga na cikhalidwe ca panthawiyo , zikhulupililo za cipembedzo , na zofuna za anthu amene ajambulitsa zithunzi zimenezo . Pa mpikisano umenewo , ndinapata mphoto yondilipilila maphunzilo pa sukulu ina yaikulu yophunzitsa kuvina yocedwa The Royal Ballet School . M’malomwake , muzisankha nkhani zimene siziloŵelela m’ndale . KODI LAFIKA PAKUTI SILINGAKONZEDWENSO ? 3 ‘ Muzikwanilitsa Zimene Mwalonjeza ’ Ndiyeno , Timoteyo anayamba kuphunzila mmene Paulo ndi Sila anali kupelekela malangizo atsopano ocokela ku bungwe lolamulila ku Yerusalemu , ndiponso mmene anali kulimbitsila cikhulupililo ca ophunzila ku Ikoniyo . 149 : 4 . Iwo analalikila anthu mamiliyoni m’maiko ambili pogwilitsila nchito zithunzi zokongola za seŵelo limeneli ndi mau ake . Pofotokoza zimene Mulungu adzacita , wamasalimo anati : “ Inu mwatembenukila dziko lapansi kuti mulipatse zinthu zoculuka , mwalilemeletsa kwambili . ” N’cifukwa cake mtumwi Yohane analemba kuti : “ Amene sakonda m’bale wake amene amamuona , sangakonde Mulungu amene sanamuonepo . ” Idzafotokozanso mmene munthu amadziŵila kuti ayenela kudya zizindikilo zimenezo . Lipoti lina la mu Nsanja ya Mlonda ya ku Finland inati : “ Timaonetsa zithunzi zimenezi kulikonse . ” Tingalimbitse bwanji cikhulupililo cathu ? ( Aroma 3 : 23 , 24 ) Kodi Paulo anatanthauza ciani pamene anakamba kuti “ kukoma mtima kwakukulu ” ? Nkhani yoyamba idzatithandiza kudziŵa mmene tingaonetsele cikondi ceni - ceni kwa anthu a kumaiko ena amene amasonkhana nafe . Koma muyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ndimakhulupililadi kuti mapeto a dzikoli ali pafupi kwambili ndi kuti zimene zikucitika padziko zimatsimikizila mfundo imeneyi ? ’ TSIKU lina pa Sondo m’maŵa mu 33 C.E . , ku Yerusalemu kunacitika zinthu zapadela komanso zosangalatsa . Tikamacita zimenezo timaonetsa kuti ndife ofunitsitsa kupewa mzimu woipa wa dziko la Satanali . Panthawiyo , dziko la Hungary linali kulamulidwa ndi boma la Cikomyunizimu . Conco ndinayamba kuphunzila Baibulo ndi m’nzanga amene anali wa Mboni . ” — José , Brazil . 8 , 9 . ( a ) Ngakhale kuti Paulo anacitilidwa zinthu zoipa ku Filipi , panakhala zotulukapo zabwino zotani ? Baibo imati : “ Munthu wokonda siliva sakhutila ndi siliva , ndipo wokonda cuma sakhutila ndi phindu limene amapeza . ” Iye pamodzi ndi hachiyo anali kuyenda pang’onopang’ono m’migodi yamdima atanyamula miyala ya malasha kucotsa pansi mamita 500 . Yehova ni woona mtima . Ifenso tili na mwayi wosankha kulambila Yehova . Mboni za Yehova zopitilila 8 miliyoni , zimalalikila na kucitila umboni uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu padziko lonse lapansi , m’maiko pafupi - fupi 240 . Anayamba kuitanila pa dzina la Yehova , koma osati monga olambila oona a Mulungu . Mateyu analemba kuti : “ Yakobo anabeleka Yosefe . ” Iye anagwilitsila nchito liu la Cigilika poonetsa kuti Yakobo anali atate a Yosefe omubeleka . Anali kucita izi potsatila miyambo yawo . Buku imeneyo inafotokozanso kuti : “ Anapanganso malamulo okhudza mabeseni oikamo madzi amene anafunika kuseŵenzetsa , mtundu wa madzi ogwilitsila nchito , munthu amene anafunika kusambitsa wodetsedwa , ndi mbali ya manja imene inayenela kusambitsidwa . ” Tidzakambilana zinthu ziti zimene zidzacotsedwa Ufumu wa Mulungu ukadzabwela ? Njila ina imene timaonetsela kuti timayamikila Yehova potipatsa mwayi wokhala naye pa ubwenzi wapadela , ni mmene timacitila zinthu na Akhristu anzathu . ( b ) Nanga zosoŵa zao zakuthupi zinasamalilidwa motani ? Kumvela cenjezo kunawapulumutsa . Mu 33 C.E . , Yesu ataukitsidwa anaonekela ku gulu la anthu oposa 500 , amene anaphatikizapo amuna , akazi , mwinanso ngakhale ana . Mfumu yaciiguputo dzina lake Thutmose Wacitatu , akuti inagwila akaidi 90,000 pambuyo pomenya nkhondo ku Kanani . Kuti apange cosankha cimeneci , io ayenela kumvetsetsa zinthu ndi kukhala ofunitsitsa kutumikila Yehova . Ngakhale kuti zinali conco , kodi iye anacita motani ? NYIMBO : 65 , 26 Ngakhale n’conco , io amadziŵa nkhani zocepa za m’Baibulo mwinanso sazidziŵa n’komwe . Mfundo imeneyi ndi yoona . Tinapeza mtendele umenewo cifukwa copemphela kwa Yehova . A Zimba : Mudziŵa bwanji kuti ulosiwo uli ndi kukwanilitsidwa kwaciŵili kumene kukukhudza Ufumu wa Mulungu ? “ Ambuye wathu Yesu Khristu mwiniyo , ndi Mulungu Atate wathu , amene anatikonda ndipo amatilimbikitsa m’njila yosalephela ndiponso anatipatsa ciyembekezo cabwino , mwa kukoma mtima kwakukulu , alimbikitse mitima yanu . ” — 2 Ates . ‘ Pitilizani Kukonda Abale ’ Jan . Ndi mafunso anai ati amene tidzakambilana pamene tikupenda mafanizo 7 a Yesu ? Kodi banja lina lacikulile linawonjezela bwanji zocita mu ulaliki wawo ? Olemba mabuku ambili amakayikila ngati fanizo limeneli linali kukamba zinthu zimene zinali kucitikadi . Kukhala ndi nkhawa zambili kumacititsa munthu kukumana ndi mavuto kapena kupanikizika maganizo kwambili , cimene cingakhale cizindikilo cakuti munthuyo ali ndi vuto lalikulu . ( Ŵelengani Nyimbo ya Solomo 5 : 12 . ) Zofalitsa zathu zonse zimazikidwa pa Baibulo . Maphunzilo . Mofanana ndi atumiki a pa Beteli , naonso amasonkhana nthawi zonse ndi kutengako mbali mu nchito yolalikila . Mpingo umapindula kwambili kukhala ndi abale ndi alongo amenewa . M’bale Mumba : Kodi mungakonde kuti ndikuonetseni mavesi a m’Baibulo amene akamba kuti kukhulupilila Yesu n’kofunika ? ( Mateyu 6 : 11 ) Yesu palembali anaonetsa kuti tiyenela kudalila Mulungu kuti atipatse cakudya ca tsiku ndi tsiku . — Salimo 37 : 25 . NYIMBO : 56 , 89 “ Ndinali kukonda kuchova njuga kwambili . ( Luka 12 : ​ 32 , 35 , 36 ) Komanso , mtumwi Paulo ndi mtumwi Yohane mouzilidwa anayelekezela otsatila a Kristu odzozedwa ndi anamwali oyela . ( 2 Akor . 5 : 6 , 11 - 13 . Koma Yobu , amene anakhalako kale - kale m’ma 1400 B.C.E . , anati za Mlengi , “ anakoloŵeka dziko lapansi m’malele . ” — Yobu 26 : 7 . Iye afunika kukonda malangizo ndi mfundo za Mulungu . Tsiku lina ndinaŵelenga ulaliki wochuka wa Yesu wa pa Phili . Ngakhale kuti onse atatu anali Akristu obatizidwa , anali kuona kuti n’zosatheka kusintha . Tsiku lina , Milan , mng’ono wake , makolo ake , ndi Mboni zina anali pa ulendo wa pa basi wocoka ku Bosnia kupita ku Serbia . 7 “ Khulupilila Yehova Ndipo Cita Zabwino ” Anthu ambili a ku Japan akamva liu lakuti “ Baibulo ” amaganizila za Yesu Kristu . Munafunsa cifukwa cake ife a Mboni za Yehova timakhulupilila kuti Ufumu wa Mulungu unayamba kulamulila mu 1914 . Koma , Yesu anatiphunzitsa kuti tifunika kufuna - funa Ufumu coyamba . Iwo anaona kuti analibe kothaŵila . ( Onani cithunzi cili kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) N’cifukwa ciani Mose anasankha kuzunzidwa pamodzi ndi anthu a Mulungu ? NYIMBO : 83 , 129 Mofanana ndi Samueli , akulu aluso masiku ano amacita zinthu mokoma mtima pophunzitsa ena . Cimene anali kutanthauza n’cakuti , ngati tiŵelengela mwininyumba Mau a Mulungu mu ulaliki , ndiye kuti tikulola Yehova kukamba naye . Mofanana na Yehova , na ise timaona anthu kukhala amtengo wapatali . Nanga ife tingamutsanzile bwanji ? Kumbukilani kuti pamene Mdyelekezi anayesa Yesu kuti asandutse miyala kukhala mitanda ya mkate , Kristu anakana kugwilitsila nchito mphamvu zake zozizwitsa kuti akhutilitse zofuna zake . ( Mat . Akhiristu ofikapo kuuzimu angathandize acatsopano kupita patsogolo mwa kuwapatsa “ malangizo abwino . ” — Miy . Iye anakamba kuti angalole kuseŵenza ngati adzayamba kugwila nchito maola ocepa ndiponso ngati adzayamba kumupatsa mpata wocita zinthu za kuuzimu . Nthawi zina , tingathe kumvetsa mavuto a ena ngakhale kuti sitinakumanepo nao . N’zoona kuti ocimwawo amakhala kuti anaononga ubwenzi wao ndi Yehova , ndipo angaone kuti n’zovuta ndiponso zocititsa manyazi kubwelela . Kuonjezela apo , mbili ya anthu yakhala yapadela . Andrés wa zaka 67 , anafotokoza kuti : “ Zikuoneka kuti Jairo amamvetsa ziphunzitso za m’Baibulo kuposa ineyo . ” Kodi mwana ameneyu anali ndani ndipo ndi liti pamene anakhala Mfumu ? YEHOVA ANASANKHA MFUMU YATSOPANO Patapita zaka 400 , Cilamulo ca Mose cinanena kuti munthu asalande mphelo kukhala monga cikole cifukwa kucita zimenezo kunali ngati “ kumulanda moyo . ” Zoona , tifunika ‘ kuganizila mozama ’ citsanzo ca kukhulupilika kwa Yesu pokumana na mayeselo osiyana - siyana . ( a ) Kodi kukonda zinthu zauzimu kwa Danieli pamene anali wacicepele kuonetsa kuti analeledwa bwanji ? Tinafika powakonda ngako anthu a mu Africa moti tinali ofunitsitsa kukabwelanso . Ndi nchito iti imene Mulungu anapatsa gulu lake latsopano ? Mukamayesetsa kuganiza ndi kucita zinthu zimene Yehova amafuna , cidzakhala copepuka kwa inu kuyamba kuona zinthu mmene iye amazionela ndi kucita zinthu zoyenela . — Salimo 37 : 31 ; Miyambo 23 : 12 ; Agalatiya 5 : 16 , 17 . Kodi cenjezo limeneli silikukumbutsani mavuto amene Aisiraeli anakumana nawo m’cipululu ? ( b ) Kodi M’bale Russell anayamba bwanji kufuna - funa coonadi ? 3 : 10 ) Tikakulitsa makhalidwe a cipatso ca mzimu cimeneci , ubale wathu ndi anthu ena umakulanso . Nzelu zanu ndi ulemelelo wanu zaposa zinthu zimene ndinamva . ” ( 1 Maf . Kodi colinga ca Mkristu aliyense n’ciani ? 8 : 38 , 39 ) M’malomwake , ngati Mkhristu mnzathu watilakwila , tiyenela kutengela citsanzo ca Yosefe . Tiyenela kuyandikila kwambili Yehova ndi kuyesetsa kuona zinthu mmene iye amazionela . Yehova anacotsa mzimu wake pa Sauli , ndipo nthawi zambili anali kuvutitsidwa ndi mzimu woipa . Tsopano , nyumba yanga ndi yaukhondo . Ngakhale zinali conco , anthu ambili otsindikiza Mabaibulo anatengela mmene Estienne anagaŵila mavesi m’Baibulo . Yelekezelani kuti muchaya nsolo ndipo mnzanu wa m’cikwati ali ku timu ina . Wophunzila Baibulo wina ku Fiji anafunika kusankha kaya kupita ku msonkhano wa cigawo , kapena kupita na mwamuna wake ku cikondwelelo ca tsiku la kubadwa la wacibale . Mwanayu amachedwa “ Mau ” cifukwa anali wolankhulila wa Mulungu wamkulu . Yesu watumikila Yehova kwa zaka zambili . Ndinayamba kuphunzila Cingelezi kuti ndionjezele utumiki wanga . Kutsatila malangizo a pa zikwangwani zimenezo kwapulumutsa miyoyo ya anthu ambili . Ndimaona kuti ndi mwai kutumikila pamodzi ndi abale amene saiwala cikondi cao coyamba kwa Yehova . Nthawi zambili , Amai ndi Atate ndi amene amacita zimenezi . 16 : 2 ) Umu ni mmene anthu amene anapha wophunzila wa Yesu , Sitefano , anali kuganizila . Ndipo pali enanso amene anacita zofanana ndi zimenezi . ( Mac . N’cifukwa ciani anaimasulila ? Zilembo zimenezi zimapezeka m’mipukutu yakale ya Ciheberi monga Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa . Patapita nthawi yocepa , Petulo anayamba kumila . Acikulile amenewa amaona kuti thandizo limene Tony ndi Wendy amapeleka ni mphatso yocokela kwa Yehova . N’cifukwa cake Baibo imati , “ palibe dzina lina pansi pa thambo , limene lapelekedwa kwa anthu , limene tiyenela kupulumutsidwa nalo . ” — Mac . 4 : 12 ; Aef . Anachulanso kuti idzaculuka , idzakhala mafumu olamulila , idzaononga adani onse , ndi kuti mitundu yonse idzadalitsidwa kupyolela mwa mbeu imeneyo . Tinasintha umoyo wathu kuti tiyandikile kwambili Mulungu kupyolela mwa Kristu Yesu . Yehova amadziŵa kuti zimene Mdyelekezi anakamba n’zabodza . Ndani apatsidwa nchito yolalikila ? Caciŵili , dziŵani kuti kudziona mosayenela kungakhale konyenga . Muziyesetsa kuzindikila mfundo zatsopano . Inu makolo , yesetsani kuthandiza ana anu mwauzimu kuti mupeze cimwemwe cimene cimabwela pamene ana asankha kukhala atumiki a Yehova odzipeleka na obatizika . Iye anati : “ Zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inuyo muwacitile zomwezo . ” Kodi kuganizila tanthauzo la zizindikilo za pa Cikumbutso kungatithandize bwanji kulimbitsa mgwilizano ? Ngati mwana wanu wacita cinthu cimene cakukhumudwitsani , musakambe kuti iye ndi munthu woipa , kapena ndi wosamvela . 7 Mmene Angelo Angakuthandizileni 33 : 12 . 5 : 4 , 5 . Koma posapita nthawi , ndinabwelelanso ku Ulaya kukakonzetsa njinga yamoto imeneyo . Baibulo limati : “ Olungama adzalandila dziko lapansi , ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya . ” — Sal . ( Salimo 63 : 6 ) Yesu amene anali wangwilo , anasankha malo acete kuti asinkhesinkhe ndi kupemphela . — Luka 6 : 12 . Koma kodi Mulungu anaonetsa bwanji cisomo cimeneci ? Mulungu ndi wokonzeka ndipo ndi wofunitsitsa kutiyanja monga anzake apamtima , ngakhale kuti ndife opanda ungwilo . ( Yes . Kucita zimenezi , kudzathandiza kwambili kuti Mau a Mulungu awafike pamtima anthu amene tikamba nawo . — Ŵelengani Luka 24 : 32 . ( Gen . 8 : 20 ; 12 : 7 ; 26 : 25 ; 35 : 1 ; Eks . Koma panopa sakucitanso mantha . ( Miyambo 12 : 1 ) Iwo ‘ amagwila malangizo , ndipo sawataya . ’ Nkhaniyo inapitiliza kuti : “ Dziŵani kuti zimene mwana wanu akucitazo sizikusonyeza kuti akudana ndi zimene mumakhulupilila . Kodi zimandivuta kukhululukila ena ? Baibulo limafotokoza mapangano 6 ogwilizana ndi Ufumu wa Mesiya , amene wolamulila wake ndi Kristu Yesu . Ngakhale kuti sitili pansi pa Cilamulo ca Mose , malamulo ake amatithandiza kudziŵa zimene Mulungu amavomeleza ndi zimene savomeleza . Nadia anakamba kuti : “ Pang’ono m’pang’ono tinacepetsa katundu wathu cakuti tinangotsala na katundu wokwana m’masutukesi anayi . ” Anthu ambili angavomeleze kuti umoyo wofotokozewa m’Baibo umene talonjezewa kutsogolo ni wabwino maningi . 26 : 53 . Ngakhale otsatila ake amene anali anzake panthawi ina anaonetsa mzimu wodzikuza ndi wodzikonda . Kucita zimenezi kungawathandiza kupitiliza kucita utumiki wawo mokondwela . ( b ) Kodi tifuna kupeza yankho pa funso iti ? Iwo ni adani a anthu ndipo acititsa mavuto ambili pa dziko lapansi . Koma pa nthawi imodzi - modzi , iye angakhale kuti ni wacangu mu ulaliki ndipo amapezeka pa misonkhano nthawi zonse . Izi zitanthauza kuti wofalitsa mmodzi afunika kulalikila anthu 28,000 m’dzikoli . Zimene anthu amakamba na kucita popeleka moni , zimasiyana malinga ndi madela amene amakhala . Yesu analonjeza abale ake adzozedwa kuti : “ Amene wapambana pa nkhondo ndi kutsatila zocita zanga kufikila mapeto , ndidzamupatsa ulamulilo pa mitundu ya anthu . Iyeyo adzakusa anthu ndi ndodo yacitsulo , ngati imenenso ine ndailandila kwa Atate wanga . Anthuwo adzaphwanyidwa - phwanyidwa ngati mbiya zadothi . ” ( Chiv . Kukamba mwacidule , sitidziŵa . Julian anakamba kuti atacotsedwa nchito anali na nkhawa yaikulu . M’masiku ovuta ano , tonse tifunika kukulitsa mzimu wa kupilila . M’bale wina wa ku Turkey anati : “ Franz Reiter anali m’bale wacinyamata amene anaphedwa cifukwa cokana kuloŵa m’gulu la asilikali a Hitler . Bwanji ponena za inuyo ? ( 1 Akorinto 4 : 17 ) N’cifukwa cake , Paulo anafuna kuti mnzake akhale pafupi naye pamene anatsala pang’ono kufa . 15 : 14 ) Mulungu anaona kuti , mbali yaikulu , Asa anam’tumikila mokhulupilika mogwilizana ndi zimene iye amafuna . Zimenezi zacititsa kuti padzikoli pakhale mavuto ambili , cisoni , ndi masoka . ( Yer . N’zotonthoza kwambili kudziŵa kuti akufa ali m’tulo m’manda ndipo sakuvutika . Pokamba za mwambo umenewu , Yesu anati : “ Muzicita zimenezi pondikumbukila . ” ( Yesaya 11 : 9 ) Ngakhale masiku ano , anthu mamiliyoni ambili azikhalidwe zosiyanasiyana ndiponso a moyo wosiyanasiyana ayamba kale kuphunzila za mfundo zapamwamba za Mulungu . Heinrich Gleissner , amene anali mmodzi wa akaidi . ( 1 Mbiri 8 : 33 ; 9 : 39 ) Pulofesa Yosef Garfinkel , amene anagwila nawo nchito yofukula mapalewo , anati : “ N’zocititsa cidwi kuona kuti dzina lakuti Esibaala lipezeka m’Baibo ndiponso m’zolemba zakale , panthawi ya ulamulilo wa Mfumu Davide cabe . ” Pa nkhani ya kukhala ogwilizana , kodi tikuphunzila ciani pa zocita za Akristu a m’nthawi ya atumwi ? 21 , 22 . Ngati musinkhasinkha zimene Yehova anakucitilani mwa kukupatsani nsembe ya dipo ya Yesu , mudzapitiliza kuyamikila ubwenzi wanu ndi Mulungu . Tatyana anafotokoza kuti : “ Popeza kuti ndinalibe nyumba yangayanga , ndinafunika kukhala m’nyumba ya lendi . Onani Nsanja ya Mlonda July 1 , 2013 , tsamba 13 ndi 14 . ( Tito 1 : 5 ) Mofananamo , Timoteyo , amene anali kuyenda ndi mtumwi Paulo pa maulendo aatali , ayenela kuti anapatsidwa udindo umodzimodziwo . ( 1 Tim . Kuyankha mwaukali kumakulitsa vuto , cifukwa kumakhala ngati kukolezela moto . ( Miy . ANTHU ambili amakamba za makhalidwe ocititsa cidwi amene anthu a Yehova ali nawo . Mwina muganiza zosamukila mumzinda wina kapena m’dziko lina kumene muona kuti mukapeza ndalama zambili ndi kukhala na umoyo wabwino . Ngati n’conco , kodi munaipemphelela nkhaniyi ndi kuganizila mmene kusamukako kungakhudzile banja lanu ndi mpingo ? Makhalidwe amenewa adzakuthandizani ngati boma lacita zinthu zacinyengo kapena zopanda cilungamo . Mukacita zimenezi mudzawathandiza kupanga zosankha . Kaya munthuyo anatilakwiladi kapena ayi , tiyenela kukumbukila kuti kukamba zinthu zimene zingaipitse mbili yake sikungathetse vutolo . ( Rute 1 : 22 ; 2 : 14 ) Masiku ano , mkate wa pita umapangidwa kwambili ku Betelehemu . Ndiloleni kuti ndikufotokozeleni . Ataganizila kuti banja lacikulile limeneli linatumikila Yehova mokhulupilika kwa umoyo wawo wonse , anadzipeleka kuti aziwasunga . Conco , amene analankhula kupitila mwa njoka anali Satana Mdyelekezi , mwana wauzimu wa Mulungu . Ndipo iye anakulitsa cikhumbo cofuna kudziimila payekha ndi kuti nayenso azilamulila . Pamene io anali kulalikila poyela , Paulo anaona mwamuna wina wolemala amene anali ndi cikhulupililo colimba . Mwacitsanzo , Yesu anali wangwilo komanso wamphamvu cakuti kulibe mwamuna wamphamvu amene angalingane naye . Iwo anali na mwayi wophunzila za cikondi cimene Mulungu anationetsa mwa kupeleka dipo . — 1 Yoh . 4 : 9 . Komabe , mudzakondwela kudziŵa kuti nkhani zimenezi zinathetsedwa mwamtendele pakati pa abale na alongo amenewa . Iwo anagwilitsila nchito malangizo a m’Baibo . Mlongo wina wa ku Spain , nayenso ali na vuto monga limeneli . Iye anati : “ Nthawi zina nimalimbana ndi maganizo ozonda anthu a mtundu wina , ndipo nthawi zambili nimakwanitsa kugonjetsa maganizo oipawo . ( Mateyu 5 : 3 ) Kaamba ka zimenezi , anthu omvela angathe kukhala mbali ya banja la Mulungu , “ ana ” ake . — Aroma 8 : 19 - 21 . Mabiliyoni a anthu amene alipo ndi moyo masiku ano , ndi mbadwa za anthu 8 aja amene anayanjidwa ndi Yehova . — Gen . Mofananamo , pamene kum’maŵa kwa dziko la Japan kunacitika civomezi camphamvu cimene cinapangitsa kuti kucitike tsunami , abale ndi alongo athu anavutika kwambili . Ndipo ici n’cifukwa cacikulu cimene timagwilitsila nchito dzina la Mulungu kwambili . Mwacionekele , iye anaphunzila luso losiyanasiyana , zinthu zakuthambo , masamu , ndi sayansi . ( Mac . Baibo ili na “ uthenga wabwino ” wopita “ kudziko lililonse , fuko lililonse , cinenelo ciliconse , ndi mtundu uliwonse . ” — Chivumbulutso 14 : 6 . Nanga mungacite ciani ngati muona kuti zikukuvutani kujaila ? ( 2 Akorinto 11 : 23 - 29 ) Komabe , Paulo sanabwelele m’mbuyo , ndipo ena analimbikitsidwa ndi citsanzo cake . Ambili amaganiza conco . 1 , 2 . ( a ) Pali umboni wanji woonetsa kuti anthu amafunafuna kukhala na ufulu ? Ndi iko komwe , kacisiyo anali “ waulemelelo wosaneneka , ” ndipo panthawiyo Solomo anali “ wamng’ono komanso wosakhwima . ” 4 : 23 , 24 ; Maliko 5 : 25 - 29 ) Yehova sanaone kuti zimene Yesu anacita n’zozizwitsa . Iwo anaipemphelela kwambili nkhaniyo , ndipo anali kuŵelenga nkhani zokhudza amishonale , ndi kulembelana ma imelo ndi abale amene anasamukila ku Taiwan . Anagulitsa magalimoto ndi katundu wao , ndipo patapita miyezi itatu anapita ku Taiwan . Komanso , amazindikilanso zolakwa zake na kuzivomeleza . Pilato atatsimikizila kwa kapitawo wa asilikali kuti Yesu wafa , anamulola Yosefe kukacotsa mtembowo . Tiyenela kuwathandiza mwaulemu ndi moleza mtima abale na alongo amene akukumana ndi mavuto ngati amenewa . — Afil . 1 : 12 - 14 ) Popeza kuti mwamuna wa Jowana anali kapitawo wa Herode , zioneka kuti iye ndi amene anali kuuza Luka zinthu zacinsinsi zokhudza Herode Antipa . Cina , Luka ndiye yekha wolemba uthenga wabwino amene anamuchula mwacindunji kuti , Jowana . — Luka 8 : 3 ; 9 : 7 - 9 ; 23 : 8 - 12 ; 24 : 10 . Taganizilani cocitika cina ici : Yelekezelani kuti wacibale wanu wacotsedwa mumpingo . Atate anga opeza anandicotsa pa nyumba yao cifukwa cakuti sanali kufuna kukhala ndi wa Mboni . Imwe acicepele acikhristu timakuyamikilani ngako cifukwa olo kuti mukukumana na mavuto , mukupitiliza kuika mtima wanu wonse pa kutumikila Yehova . Conco , zimene atumwi anacita zionetsa kuti mpingo ungathandize kusamalila osoŵa . Ndinali ndisanatsogozepo phunzilo lokhazikika . Conco , ndinaganiza kuti a Doris angayenelele kuphunzila ndi mlongo wokhwima , mwina wa msinkhu wao . ” Komatu osati mwa kufuna kwanga , koma mwa kufuna kwanu . ” Yesu anaikidwa mwacindunji kuti akhale wansembe kupitila mu pangano limene Yehova anacita ndi iye . Ndipo iye adzakhalabe “ wansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melekizedeki . ” ( Aheb . M’nthawi yakale , Asukuti anali kuonedwa ngati anthu otsika ndi otsalila . Pa cifukwa cimeneci , mneneli ameneyu anapulumutsidwa “ kwa mikango . ” — Dan . Iye anayankha mosapita mbali kuti : “ Aliyense wosiya mkazi wake n’kukwatila wina wacita cigololo , kupatulapo ngati wamusiya cifukwa ca dama . ” — Mateyu 19 : 6 , 9 . Tikacita izi , Mulungu adzalandila ulemelelo . — 1 Akor . Koma cimene cinapangitsa Baibo imeneyi kukhala yofunika kwambili , n’cakuti inali kuthandiza kwambili ana a sukulu kuphunzila Ciheberi . Enanso angavutike kuti akhululukile munthu amene anawakhumudwitsa kapena kuwalakwila . Ndiye kodi kuloŵelelapo pankhaniyi sikukanangopangitsa kuti Natani asokoneze ubwenzi wake ndi Davide , umene unakhalapo kwa nthawi yaitali ? Conco zimadalila munthu aliyense payekha kudziika mwadala pa mayeselo kapena ai . Iwo anayamba nchito yaikulu yolalikila panthawi imeneyo . ( Luka 6 : 45 ) Pokambilana ndi ena , tidzapewa kukamba kwambili pa zinthu zimene tacita ndi maudindo amene tili nao . Koma kodi ‘ mungafutukule mtima wanu ’ mwa kuwonjezela zimene mumacita polimbikitsa abale na alongo ? — 2 Akor . 6 : 11 - 13 . Nsanja ya Mlonda iyi , ifotokoza mmene mungapindulile cifukwa cakuti Yesu anavutika ndi kutifela . Kodi sadzaganiza kuti ndise asilikali ? ” Kukhala ndi mtima woyamikila kungatithandize kupilila mavuto aakulu . Tidzaphunzilanso zimene zingatithandize kuti tizidalila citsogozo ca Yehova . Kodi Yefita analonjeza ciani ? Nanga panakhala zotulukapo zanji ? Iye anali asanamangepo cingalawa . Tiyenela kuganizila ciani posankha zimene tifuna kuvala ? Kodi mungakonde kudziŵa zinthu zina zimene Baibulo imakamba ndi kuziyelekezela na zimene mumaphunzila kuchechi kwanu ? Mofananamo , mungathe kuona zinthu za m’dziko ndi kudziŵa Mulungu wosaonekayo amene analenga zinthuzo . Cifukwa ca mmene tuakacisito amatukonzela , Akristu oona amapewelatu kulambila pa malo amenewo . Koma n’zacisoni kuti amtolankhani ambili a m’dzikoli amanyalanyaza kuuza anthu nkhani zofunika kwambili za mbili ya anthu . Zimenezi zinacititsa kuti mpingo wonse ukhale na cisoni . Ambili amabatizika ali acicepele , ndipo amakula ndi kukhalabe okhulupilika kwa Yehova . Anthu ena amakhulupilila kuti . . . n’zosatheka kukhala na mtendele weni - weni wa m’maganizo m’dziko lino lodzala ndi mavuto na kupanda cilungamo . DZIKO : COSTA RICA Kodi mphamvu imeneyo tingaigwilitsile nchito bwanji ? Ndiyeno , anali kuyembekezela kwa mawiki ambili kuti zitsulo zagalimoto yowonongekayo zibwele . M’nyumba zina mmene tinali kukhala zimbudzi zinali za panja , ndipo munali kuzizila kwambili . ( Yohane 7 : 10 , 11 ) Iye sanali kuoneka mosiyanako ngakhale pakati pa atumwi ake 11 okhulupilika . Kumbukilani kuti iye “ [ Mulungu ] safuna kuti wina aliyense adzaonongedwe , koma amafuna kuti anthu onse alape . ” Cifukwa cacitatu cimene timakhulupilila kuti Yesu anaukitsidwa n’cakuti ophunzila ake analalikila mwacangu za kuuka kwake . Koma iye sanalole lamulo la mfumu kumulepheletsa kukwanilitsa udindo wake wa M’malemba wopemphela . Pangano lina likutsimikizila kuti zimenezo n’zosatheka . Pa ulaliki wake wochuka wa pa phiri , Yesu anati : “ Winawake waudindo akakulamula kuti umunyamulile katundu mtunda wa kilomita imodzi , umunyamulile mtunda wa makilomita aŵili . ” Tikamaŵelenga Baibulo tsiku ndi tsiku , timapeza nkhani zimene zingatithandize kugonjetsa zizoloŵezi ndi zilakolako zoipa . Citsanzo cina ni ca mlongo wa ku Colorado , m’dziko la United States , amene ni mpainiya . Analinso kufunafuna anthu kunyumba zao . ( 3 ) Kupewa kukangana ndi mwininyumba . Anali kukhala na mayanjano abwino ndi otsitsimula monga mafuta odzozela munthu . Umakamba za loto limene Mfumu Nebukadinezara wa ku Babulo analota . Kumatithandizanso kupewa kudzikweza ngati anthu ena atilemekeza . Kenako , tinamupangila tiyi na cokoleti . Zimenezi zinathandiza kuti ubwenzi wawo na anthu a mumpingo watsopano ulimbe . 5 : 17 ) Kuti athandize zolengedwa zake zanzelu kukhutila ndi kukhala ndi cimwemwe cimene iye ali naco , Yehova amagaŵila zolengedwa zake nchito yabwino ndi yokondweletsa . Pofotokozela munthu cigamulo cao , io ayenela kukamba mokoma mtima ndi kumufotokozela momveka bwino zimene afunika kucita kuti adzabwezeletsedwe mumpingo . Cosankha cimene mungapange , kaya ndi cokhudza cikwati kapena nchito cingakhudzenso utumiki wanu kwa Mulungu . ( Yobu 1 : 18 , 19 ; 2 : 7 , 9 ; 19 : 1 - 3 ) Yobu sanali kudziŵa cifukwa cake anali kukumana ndi mavuto ambili , koma anakhalabe wokhulupilika . Imakhutilitsa colaka - laka cathu . ( Yoh . 13 : 7 ) Tingaonetse kuti timalemekeza ena mwa kupewa kudziona monga ndise ofunika ngako cifukwa ca maphunzilo athu , cuma , kapena utumiki na udindo umene tili nawo m’gulu la Yehova . Kodi iye anali na ciyembekezo cakuti adzaukitsidwa ? Kupeleka ziwalo zathu mu ukapolo ku cilungamo sikutanthauza kungopewa cabe kukolewa , koma ngakhale kupewa kumwa moŵa motsala pang’ono kukolewa . Inunso kungakuthandizeni kukhala wacimwemwe . Ndipo cimene cinawonjezela vuto n’cakuti anthu okhometsa msonkho anali acinyengo . Yosimbidwa ndi Annunziato Lugarà 5 : 28 , 29 ) Idzakhala nthawi yosangalatsa zedi kulandila okondedwa athu amene adzaukitsidwa . Tinganene kuti Yosefe anali kufunika kucita zinthu monga mmene aneneli amene anadzakhalapo ndi moyo anali kucitila pofotokoza mauthenga a Mulungu ndi ziweluzo Zake kwa anthu ake osamvela . Si apo pokha . Iye anakhala m’tauni ya Asamariya kwa masiku aŵili cifukwa cakuti anthu a kumeneko anali kumvetsela mwacidwi uthenga wake . — Yoh . 4 : 21 - 24 , 40 . Lomba tiyeni tikambilane zimene tingacite kuti tipitilize kukonda Ufumu wa Mulungu , ulaliki , ndi coonadi . Kuyelekezela kwa mtundu umenewu kungathandize mwana wanu kuona kuti Yehova analembelatu kale - kale m’Baibulo zinthu zoona zimene zatengela anthu zaka zambili - mbili kuti apeze umboni wake . — Neh . Pamene tikupilila ciyeso , timayamba kuonetsa kwambili makhalidwe amenewa . Mwanjila imeneyi , kupilila kumatithandiza kukonza umunthu wathu . Sukuluyi inakhala mphatso yosaiwalika yocokela kwa Yehova . ” Posapita nthawi tinayamba kukonda dziko la Kenya ndi utumiki wathu . Mnzakeyo anali ndi amai ake ndi ambuye ake aakazi amene anali kumuyembekeza kuti akwele ndeke yopita ku South Africa . N’naona kuti zimene dokotayo anakamba ni yankho yocokela kwa Yehova . ” Koma akafika pa zaka zovomelezeka ndi boma , amayamba kuyendetsa motokayo pamene atate wake akum’patsa malangizo a moyendetsela . Luka , sanali cabe munthu wokonda kupatsa anthu malangizo a zaumoyo . Monga kholo , n’ciani cimene mungacite kuti muphunzitse ana anu acinyamata kutumikila Yehova ? 15 : 3 - 6 ) Tifuna kuti zosankha zathu zizilemekeza Mulungu ndi mpingo . — 2 Akor . Yendani pa www . jw . org , kapena unikani kacidindo ka QR aka Munthu aliyense saloledwa kuika zofalitsa zathu pa mawebusaiti ena Wacinyamata Timoteyo anaseŵenza pamodzi na mtumwi Paulo kwa zaka zambili . Timakonda kucita zinthu zanji tsiku na tsiku ? Ambili m’dzikoli amayesetsa kubisa zocita zawo zoipa , ndipo nthawi zambili salandila cilango pa zocita zawozo . Mkwatibwi “ wakongoletsedwela mwamuna wake ” ndipo ali pa “ ulemelelo waukulu ” kaamba ka cikwati ca mfumu . Pamene muphunzitsa ena Baibulo , muzigogomezela umboni wakuti Mulungu aliko , amasamala za ife , ndiponso kuti Baibulo ndi Mau a Mulungu . Komanso akulephela kukamba , ndipo aoneka kuti angafe ngati munthu wina sangamuthandize mwamsanga . 12 Yehova Amakonda Anthu Amene ‘ Amabala Zipatso mwa Kupilila ’ Kupewa ciwelewele kumatithandiza kukhala ndi mtendele wa m’maganizo ndi kukhala osangalala . Martin Luther anali kale memba wa cipembedzo pamene anayamba kuphunzila mosamala kwambili zimene Lefèvre anamasulila . Aka kanali kacitatu kuti Jordan alephele kutsatila malamulo a pa nyumba . Mulungu adzathandiza anthu kukhalanso ndi thanzi labwino . Musafooke . Madzulo a tsiku lakuti maŵa Blossom adzabatizika , atate ake anacita cinthu cinacake cocititsa cidwi . Kodi colinga ca Mulungu cakuti anthu adzaze dziko lapansi cinasokonezeka bwanji ? Baibulo limatiuza kuti Mulungu Wamphamvuyonse amayankha mapemphelo a atumiki ake okhulupilika . Conco , cinthu canzelu cimene tingacite ni kupita patsogolo kuti tikwanilitse ziyeneletso . Zimenezo zingathandize makolo kusamalila zosoŵa za aliyense m’banja , ndipo zingawapatse mpata wosintha nkhani ndi kacitidwe kake . NYIMBO : 112 Pofuna kucepetsa nchito ya anthu okwana 576 amene anali kutsuka mbale , anthu obwela ku msonkhano anali kunyamula mipeni ndi mafoloko ao . Kodi n’ciani cinacitika pa nthawiyo ? Aisiraeli anafika pa malo amene pambuyo pake anachedwanso Meriba . Tiyenela kuonetsa mwa zocita zathu kuti tamvela ndi kumvetsetsa tanthauzo la mafanizo a Ufumu amenewa . Timayembekezela Yehova na mtima wonse cifukwa tidziŵa kuti panthawi yake yoyenelela , adzatipatsa moyo wosatha monga mmene analonjezela . Ngakhale anthu osauka angakhale ndi mzimu wokonda cuma cakuti angaleke kufuna - funa Ufumu coyamba . — Aheb . 4 : 4 , 7 , 12 . Tiyenela kukumbukila kuti kukhala na cidziŵitso ca m’Baibo pakokha , sikokwanila kuti munthu akhale wauzimu . Yankho inali yakuti : “ Ni anthu pafupi - fupi 50 ! ” Inde 7 : 4 ) Mofananamo , pa Ekisodo 14 : 21 pamati : “ Yehova anacititsa mphepo yamphamvu yakum’mawa kuyamba kugaŵa nyanjayo . ” Nili ndi zaka 18 , n’naikidwa m’ndende kwa miyezi 9 cifukwa cokana kuloŵa usilikali . Koma ngakhale n’conco , io amafunikila kuwalimbikitsa . ” Panthawiyo tinayambanso kulambila Yehova Mulungu momasuka . 24 : 15 ) Timamva cisoni kwambili munthu amene timakonda akamwalila . Koma podziŵa kuti adzauka , ‘ siticita cisoni mofanana ndi onse opanda ciyembekezo . ’ ( 1 Ates . Tifunika kumaŵelenga Baibo tsiku lililonse , na kuseŵenzetsa mosamala mfundo zimene taŵelengazo pamene takumana na ciyeso . ( Machitidwe 16 : 2 ) N’ciani cinam’thandiza kukhala ndi mbili yabwino imeneyi ? Mu 2007 , Bungwe Lolamulila linakonza zakuti masukulu amene anali kucitikila pa Beteli aziyang’anilidwa ndi Dipatimenti ya Sukulu Zophunzitsa Atumiki a Mulungu . MUNTHU akamva zimene winawake akulankhula , angazindikile kuti munthuyo wakondwela kapena ai malinga ndi mmene mauwo akumvekela . Kumbukilani kuti Yesu anadzudzula atsogoleli acipembedzo a m’nthawi yake ndi kuwauza kuti ndi atsogoleli akhungu ndi acinyengo . tili ndi zofooka ? Abale ofikapo amenewa angathandize a m’cikwati za mmene angagwilitsile nchito uphungu wa m’Mau a Mulungu . Pofuna kudzipenda kuti tione ngati timakonda anthu ena na mtima wonse , tingadzifunse kuti : ‘ Kodi nimayesetsa kuthandiza ena pa banja pathu , mu mpingo , kapena mu ulaliki ? Ndithudi , palibe mau ena amene angaticititse “ kumvela bwino ” kuposa mau oimbidwa pofuna kutamanda Atate wathu wakumwamba Yehova , na kuonetsa cikondi cathu pa iye . ( Ŵelengani Nehemiya 8 : 8 , 12 . ) Zoonadi , kaya titumikila ku dela liti , tikali na “ zocita zambili . . . mu nchito ya Ambuye . ” — 1 Akor . Koma ndimakumbukila zimene m’bale wina anandiuza kuti , ‘ Uyenela kucita zonse zimene ungathe , ndipo Yehova adzasamalila zotsala . ’ ” Iye anati : “ Anthu ambili m’gawo lathu amatilola kuŵelenga nao lemba limodzi ngati tidzakamba mwacidule ndi mosapita m’mbali . Tiyenela kukhala wosamala kuti tisatengemo mbali m’zocitika za m’dzikoli ndi kuyamba mikangano . Ndipo pamene ayang’anizana na mayeselo kusukulu , acilikizeni kwambili . Kuonjezela apo , zikhala bwanji abale ake akaona mphatso imene atate ao amupatsa ? Koma Paulo anazindikila kuti kumaiko ena kunali kusoŵa kwakukulu . Panthawiyo , n’nali na zaka 16 cabe . Kodi muganiza kuti anaseŵenzetsa malangizo ati a m’Baibo ? 77 : 12 . Senzani goli langa ndipo phunzilani kwa ine , cifukwa ndine wofatsa ndi wodzicepetsa , ndipo mudzatsitsimulidwa , pakuti goli langa ndi lofewa ndipo katundu wanga ndi wopepuka . ” Ena anali kuseŵenzetsa amkola bongo , ena anali akaidi . Mutapita kucipatala , dokota wakupatsani malangizo okhudza kadyedwe , kucita maseŵela olimbitsa thupi , na kusintha zinthu zina mu umoyo wanu . Ali pa nchito yapadela yokalalikila kwa anthu akutali pamene nyengo yakhalako bwino . Yoswa ayenela kuti anacita mantha . Kodi kudzicepetsa n’ciani , ndipo kuli na ubwino wanji ? Iye amadziŵa mmene thupi limagwilila nchito , ndipo ali na mphamvu zopoletsa matenda aliwonse . ( 1 Akor . 15 : 22 ) Pamenepa pangabuke funso limene Paulo anafunsa lakuti : “ Ndani adzandipulumutse ku thupi limene likufa imfa imeneyi ? ” ( Onani kabokosi . ) Mwacitsanzo , nkhondo yoyamba ya padziko lonse isanayambe komanso itayamba , io anali kuonetsa “ Seŵelo la pa Kanema la Cilengedwe . ” Kodi mwam’kumbukila Alexandra amene tam’chula kuciyambi kwa nkhani ino ? Mofanana ndi zimene zinacitikila Paulo na Sila ku Filipi , ifenso tingadabwe kwambili na thandizo limene Yehova angatipatse . Iwo amavomeleza zinthu zikasintha . 5 : 22 ) Conco , onse amene ali na cikhulupililo afunika kuyamikila ngako . Iye mwaulemu anacondelela Davide kuti asabwezele coipa ndi kuwononga ubwenzi wake na Yehova . 23 : 5 ) Kuthandizana mwanjila imeneyi kungacititse kuti anthu amene anali paudani akhale mabwenzi . Kodi tingapindule bwanji ndi magazini amenewa ? Kodi Yehova adzacita ciani Satana akadzafuna kuononga atumiki ake ? Nthawi na nthawi , makolo angamapemphe mabanja ena acikhristu kuti akhale nawo pa kulambila kwawo kwa pabanja . Ngati makolo anu ndi Mboni ndipo amakhala kutali ndi inu , mungakambe ndi akulu a kumpingo wao kuti mufunsile zimene mungacite . ( 2 Mbiri 15 : 16 , 17 ; 25 : 1 , 2 ; Miy . Katswili wina , John Parkhurst , anati : “ Pokamba za Mulungu kapena Khiristu , liulo [ la Cigirikilo ] nthawi zambili limatanthauza kukoma mtima kwa m’cisomo cawo kowombola na kupulumutsa anthu . ” ( Akolose 3 : 15 ) Mukalandila thandizo , muziyamikila . Yonatani anadziŵa kuti Mulungu ali ndi Davide osati Sauli , conco anasankha kukhala wokhulupilika kwa Davide . Ndinakumbukila kuti alongo ao ena a atate anali a Mboni . ( Aroma 7 : 6 ) Koma Yehova anaonetsetsa kuti Cilamulo casungiwa m’Mau ake Baibo , kuti citithandize . Anthu amene anamugula anapita naye ku Iguputo , ndipo kumeneko anayamba kutumikila m’nyumba ya Potifara . N’cifukwa ciani tifunika kupitiliza kutonthoza ena ? Fotokozani citsanzo coonetsa ubwino wokhala odzicepetsa . ( Yer . 10 : 23 ) Conde , tisagwele mu msampa wodalila nzelu zathu , monga anacitila Adamu ndi Aisiraeli opanduka aja . Tidzapeza njila zambili zolimbikitsila ena mwauzimu ngati titsatila malangizo a Paulo akuti : “ Pitilizani kutonthozana ndi kulimbikitsana monga mmene mukucitila . ” ( 1 Ates . Ngati timasankha anthu a mtundu wina kapena a dziko lina , ndiye kuti tikunyalanyaza mfundo yakuti “ kucokela mwa munthu mmodzi [ Mulungu ] anapanga mtundu wonse wa anthu . ” ( Mac . Lemba la Chivumbulutso 14 : 1 , 4 limati : “ Ndinaona Mwanawankhosa ataimilila paphili la Ziyoni . 13 : 1 , 2 ) Ngakhale Yesu Khristu Ambuye wathu , anafunsa funso limeneli poona kupanda cikhulupililo kwa anthu a m’nthawi yake . Sadziŵanso kuti cheyamani ali pa pulatifomu , nyimbo zamalimba zilila , ndi kuti anthu onse akhala pamipando yawo . Kuganizila cocitika ici kungatithandize kuona kufunika kokhala maso ku cocitika cacikulu cimene cidzacitika posacedwa . 3 : 2 ; 3 Yoh . Nthawi zonse atumiki a Yehova okhulupilika amatsatila mofunitsitsa malangizo a gulu la Mulungu . “ Pitilizani kutonthozana ndi kulimbikitsana . ” — 1 ATES . Iye anayamba kuphunzila cinenelo ca Cichaina ndi kugwilizana ndi kagulu ka Cichaina . Conco , iye anadziikila colinga cosamukila ku Taiwan , ndipo mu September 2008 , anakwanilitsa colinga cake . Mosiyana ndi cipembedzo conama , cipembedzo coona cimaona kuti ulamulilo wa Yehova ni wofunika kwambili . Nthawi zambili cimakhala ca kanthawi kocepa , zimene zingakhale zokhumudwitsa . Nthawi zambili olosela amakamba zinthu zakuti zingacitike kwa aliyense . Kodi mipingo yoyambilila yacikhristu inakhudzidwa bwanji na kalata yocokela ku bungwe lolamulila ? Ndipo timakondwela kwambili kuona anthu amene taphunzitsa ‘ akugwila nchito mwakhama ndiponso mwamphamvu . ’ Kodi Ndani Maka - maka Amacititsa Nkhondo ndi Mavuto ? ▪ Muzitsanzila Mulungu Amene Watilonjeza Moyo Wosatha N’namvela bwino kwambili . ” Zida zimene ogwila nchito ku migodi ya ku Poland ndi ya ku Dechy pafupi ndi Sin - le - Noble amaseŵenzetsa , ndipo ndi kumene Antoine Skalecki anali kuseŵenza . Anakamba kuti anthu otelo ali ngati cofufumitsa cimene cimafufumitsa mtanda wonse . Mneneli Eliya anali wokhulupilika kwa Yehova ndipo anali ndi cikhulupililo colimba . Baibulo limafotokoza kuti zocitika m’nthawi ya mapeto zidzakhala zapadela komanso zovuta m’mbili ya anthu . Conco , ziyenela kuti zinali zosavuta kwa iwo kukhulupilila mwamuna wokhwima mwauzimu ameneyu . — Aheb . Mofananamo , mbali yoyamba ya cisautso cacikulu idzafupikitsidwa cifukwa ca “ osankhidwawo . ” ( Mat . 5 : 14 - 16 ) Pokhala anthu oyela , timaonetsa mwa zocita zathu kuti malamulo a Yehova ni abwino , ndi kuti zokamba za Satana n’zabodza . Kodi mumakhulupilila kuti Yehova ndi wokonzeka kukucilikizani pamene mudwala ndi kuti ali na mphamvu yocita zimenezo ? — Sal . Kodi ineyo ndithu ndi mai akowa , komanso abale akowa tidzagwada pansi pamaso pa iwe ? ’ ” Pakuti muyezo umene mukuyezela ena , iwonso adzakuyezelani womwewo . ” Akulu angawathandize anthu amenewa kuti azimvetsela misonkhano . Angacite zimenezi mwa kulumikiza misonkhano kudzela pa foni kapena kuwajambulila misonkhanoyo . N’nakondwela ngako pamene n’naphunzila m’Baibo kuti Mulungu yekha na amene angabweletse mtendele padziko lapansi . “ Tikhale olimba mtima ndithu ndipo tinene kuti : ‘ Yehova ndiye mthandizi wanga . ’ ” — AHEB . Popeza Hagara analakwitsa , kodi Mulungu anamuiwala ? Cikondi sicitha . ” Mungaseŵenzetse zinthu zodziŵika bwino kuti muthandize ana anu kukulitsa cikhulupililo mwa Mulungu na cilengedwe ( Onani ndime 10 ) Tiziganizila mmene colakwaco cidzakhudzila umoyo wathu , okondedwa athu , ndipo makamaka ubale wathu ndi Yehova . Iye anacita lonjezo limeneli pamene anali kusautsika ndi nkhawa mumtima mwake cifukwa ca kusabeleka ndiponso cifukwa cotonzedwa nthawi zonse ndi mkazi mnzake . Pamene mayiyo analimbikila , Yesu anakamba kuti : “ Si bwino kutenga cakudya ca ana n’kuponyela tiagalu . ” Kodi ningaseŵenzetse bwanji mfundo zimenezi pothandiza ena ? ’ Kodi iye anali kuona cithunzi m’maganizo mwake ca umoyo wosangalatsa umene tidzakhala nawo cifukwa ca “ mbeu ” yolonjezedwa ? Iye anali kuponda - pondanso m’copondela mphesa ca mkwiyo waukulu wa Mulungu Wamphamvuyonse . ” — Chiv . Kucita zimenezi kudzatithandiza kuyamba kuona zinthu mmene Yehova amazionela . Ngati tifuna kokondweletsa Yehova , tifunika kutsatila kwambili malamulo ndi mfundo zake , ndipo sitiyenela kutengela khalidwe lopeputsa malamulo ndi mfundo zimenezo . ( 1 Mbiri 23 : 1 - 6 ; 24 : 1 - 3 ) Ndipo pamene Aisiraeli anamvela Yehova , anali kudalitsidwa . Pamene Adamu anacimwa , Yehova anamuweluza kuti afe . Zotsatilapo n’zakuti anthu onse anakhala opanda ungwilo ndipo amafa . Cifukwa ca ici , kunali kukhala nchito yambili . Umalimbikitsa anthu kukhala na umoyo waufulu ndi wacimwemwe . Tidziŵa kuti anthu ena angatinyoze cifukwa cokana kuikidwa magazi , koma timafuna kumvela Mulungu . Anthu ake adzakhala na umoyo wacimwemwe ndipo adzakhala naye paubwenzi wolimba , umene n’cinthu camtengo wapatali kuposa cuma cakuthupi . — Sal . Munthu amene akutsatila cilungamo afunikanso kumapezeka pa misonkhano ya mpingo ndi kutengako mbali mokwanila m’nchito yopulumutsa moyo , yolalikila na kupanga ophunzila . 2 : 7 ) Pambuyo pa imfa yake yodzipeleka nsembe , Yesu anabwelela ku moyo wauzimu kumwamba ndipo anakhala Mfumu ya Ufumu wa Mulungu mu 1914 . ( Aheb . 34 : 8 ) Lemba limeneli lionetsa ubwino wodzionela tekha thandizo la Mulungu mu umoyo wathu . Kupezeka pa Cikumbutso kudzakuthandizani kuyamikila kwambili nsembe ya dipo ya Yesu . Kodi nacita ciani kuti nikakwanitse kusamalila thanzi langa ? Iwo angakambe kuti : “ N’cifukwa ciani mumalimbitsa zinthu kwambili ? Mwamantha , n’nayamba kulalikila nyumba ndi nyumba . Mbali yothela ya lembali imati : “ Amene akufunafuna Yehova amamvetsa ciliconse , ” kutanthauza ciliconse cofunikila kuti munthu athe kukondweletsa Mulungu . Kodi makolo angacitenji kuti awadziŵe bwino ana ao ? Koma akatswili apeza kuti nthawi zambili kuculukitsa malamulo kumangopangitsa kuti anthu azicita ziphuphu kwambili . Pamimba pa msilikaliyo , pacifuwa cake , na pamapewa , monse munali kukhala tunsimbi topyapyala tomangiwa na nthambo za cikumba . Ganizilankoni zimene mungacite kuti mukhale ndi umoyo wosafuna zinthu zambili kuti muzikhala ndi nthawi yambili yocita zinthu za kuuzimu . Kugwila nchito yocepa sikubweletsa cimwemwe cokhalitsa koma kumapangitsa munthu kukhala ndi umoyo wosasangalala . ” Khazeni wanga , Nicolas Psarras , amene tinali kukhala naye pafupi , anamulamula kuti aloŵe m’gulu la asilikali a Greece . Popeza n’zosatheka kudziŵa maina a odzozedwa onse amene ali padziko lapansi , zingatheke bwanji kuti a nkhosa zina ‘ apite nao limodzi ’ ? 24 : 11 ) Nkhaniyo inagogomeza kwambili za udindo wathu wolalikila uthenga wa m’Baibo wopulumutsa moyo . ( Mac . Akristu onse amatengela citsanzo ca odzozedwa pankhaniyi , ndipo amaika utumiki wao patsogolo . Kapena cingakhale cifukwa cosungulumwa , kapenanso cifukwa codziona kuti sacita bwino mwauzimu poyelekeza na acicepele anzake acikhristu . Ndipo Yehova akamayankha mapemphelo anu , ubwenzi wanu ndi iye umalimba kwambili . 15 : 1 . N’ciani cinapangitsa anthu ena kuyamba kudzikweza ? Yesu ananena kuti mwina adzabwela “ atambala akulila , kapena m’maŵa . ” Mofananamo , tingapindule ndi zofalitsa zonse zimene gulu lathu limafalitsa . * N’nasoŵa cokamba . Nanga tingapindule bwanji ndi zocitika ndiponso zitsanzo za m’Malemba ? N’cifukwa ciani ndi anthu ocepa cabe amene anafa ? Mu 1958 , ca m’ma March kapena April , ndinali pafupi kutsiliza maphunzilo anga monga wopeleka zakudya mu hotelo ina yochedwa Grand Hotel Wiesler , m’tauni ya Graz , ku Austria . Koma anthu ena sakhala omasuka kupeleka moni , cifukwa ca manyazi kapena cifukwa codziona monga osafunika . Iye angalole kuti tisoŵe zinthu zina kuti tithandizile kuyankha mabodza a Mdyelekezi . Olemba Baibulo sanagaŵe uthenga wao m’macaputala ndi m’mavesi polilemba . Mmodzi mwa woyang’anila dela amene ananithandiza kwambili ni M’bale Jesse Cantwell ndi mkazi wake , Lynn . Tifunika kumuyamikila Mulungu kaamba ka zinthu zonsezi . Iye ndi Mlengi wathu ndipo amatisamalila . ( Yeremiya 25 : 9 , 15 - 18 ) N’ciani cinacitikila Ayuda osalakwa amene sanali kucitako zoipa mumzindawo ? 41 : 10 , 13 . ( 1 Yohane 4 : 16 ) Yesu Kristu , amene Mulungu anayambila kulenga , anakhala kumwamba ndi Atate ake kwa zaka mabiliyoni ambili . Tiyenela kusonkhana pamodzi kuti tikhale mbali ya “ gulu limodzi ” ndi kutsatila “ m’busa mmodzi . ” Kodi Yehova anam’dalitsa bwanji cifukwa colela Mwana wake mokhulupilika ? Kodi kulemekeza dongosolo la umutu kumaonetsa bwanji kuti timakonda ulamulilo wa Yehova ? M’nkhani ino , takambilana kuti tingalimbitse mgwilizano pakati pathu m’njila zitatu izi : ( 1 ) Mwa kudalila Ufumu wa Mulungu wakumwamba kuti ni umene udzathetsa kupanda cilungamo , ( 2 ) kupewa kutenga mbali m’zandale , ndi ( 3 ) kupewa kucita zaciwawa . ( Genesis 3 : 1 - 7 ; Chivumbulutso 12 : 9 ) Baibo sikamba dzina la mngelo ameneyo kapena udindo wake akalibe kupanduka . Kukula kumacitika ‘ pakokha , ’ mwapang’onopang’ono . Nthawi zina Yehova amayankha mapemphelo athu kudzela m’Mau ake , Baibulo . Fotokozani malangizo a m’Baibulo okhudza kukwatila kapena kukwatiwa kokha “ mwa Ambuye . ” Kutengela citsanzo ca Yosefe cingakhale cinthu canzelu kwambili Ngakhale kuti Yesu anali kuphunzitsa coonadi ndipo anali kudziŵa kuti cipulumutso cikucokela kwa Ayuda , sanalimbikitse atumwi ake kudana ndi mitundu ina . ( Yoh . Kukambilana ndi Munthu Wina Nkhani za m’Baibulo — Kodi Ufumu wa Mulungu Unayamba Liti Kulamulila ? 10 pakuti cinyengo cotsilizaci cidzakhala coipa kwambili kuposa coyamba cija . ” Pamene boma inawaletsa kugaŵila buku lakuti The Finished Mystery kuciyambi - yambi kwa 1918 , ulaliki unakhala wovuta kwa abale ambili . Ndinawauza kuti likulu la Mboni za Yehova limachulidwa m’Baibulo . Anadzipeleka ku Turkey , July Mwaubwenzi , Yohane anachula Gayo kuti “ wokondedwa , amene ndimamukonda kwambili . ” ( Gen . 2 : 21 - 23 ) Popeza kuti Yehova analenga anthu m’njila yakuti azisonyeza cikondi , n’zotheka kuti mwamuna ndi mkazi azisonyezana cikondi ceniceni . Mosasamala kanthu za zimenezi , Yosefe anamvela bambo ake ndipo anapita . — Genesis 34 : 25 - 30 ; 37 : 12 - 14 . MWANA woyamba kubadwa wa Mulungu ndi colengedwa capamwamba koposa cimene cimaonetsa nzelu zakuya za Yehova . Muziwapemphelela komanso kupemphela nawo pamodzi . Eliya anali kukhulupilila ndi kumvela Mulungu wake . Ndiyeno , Zekariya anaona akazi aŵili okhala na mapiko olimba ngati a dokowe . Kodi mukanakhala inu mukanacita ciani ? ( Mlaliki 3 : 7 ) Mwacitsanzo , timakhala cete pamene ena akulankhula pofuna kuonetsa ulemu . Komabe , mu 1995 , kamvedwe kathu pa fanizo limeneli kanasintha . Baibulo linanenelatu kuti ‘ m’masiku otsiliza ’ khalidwe la anthu lidzaipa . Pamene tiphunzila za makhalidwe abwino a Yehova timam’yandikila kwambili N’nabwelela ku Karachi , ndipo kenako n’napita ku London , m’dziko la England , nili na maganizo okalimbitsanso umoyo wanga wauzimu . Kodi nikutengela makhalidwe a Khristu ? Mlongo Olga , amene amakhala ku South America , anaonetsa kuti ndi wokhulupilika kwa Yehova mwa kulemekeza mwamuna wake ngakhale kuti anali kumucitila zinthu mwankhanza . Baibulo limafotokoza bwino kwambili ponena za Yesu . Cilimikani pa Kulimbana Kuti Mupeze Madalitso a Yehova , Sept . N’cifukwa ciani Marita anakamba conco ? Nanga tiphunzilapo ciani pa zimene Yesu anamuyankha ? Zingakhale zovutitsa maganizo . Ambili anaganiza zoyamba utumiki wa nthawi zonse . N’ciani cawathandiza kulankhula molimba mtima ? Tiyeni tipitilize kutengela cikhulupililo colimba ca anthu amenewa . 14 : 13 ) Kodi Yesu anacita ciani ? Tsiku lotsatila m’masitolo onse munalibe cakudya ciliconse . ” — Paul , wa ku Zimbabwe . ( Gen . 39 : 12 , 20 ) Pocoka ku khoti , dilaiva amene ananyamula Maria kupita naye ku ndende anamuuza kuti : “ Usacite mantha . N’ciani cingathandize kuti banja liziyenda bwino ngakhale kuti ndife opanda ungwilo ? Malangizo amene timalandila pa msonkhanowu amatithandiza kudziŵa bwino mocitila maulendo obwelelako ndi mocititsila maphunzilo a Baibo . Zinali zosatheka kuphunzitsa ana anga poonekela , kapenanso kupita nao kumisonkhano . ” Conco , olo kuti sitidziŵa zambili , n’zoonekelatu kuti Yesu sanali kuoneka monga mmene anthu ambili amamuonetsela . Maria anawamvela cifundo podziŵa kuti anali kucita izi cabe cifukwa comvela malamulo . Ngati ndife odzicepetsa ndipo timagwilizana ndi akulu , mpingo wathu udzakhala wogwilizana ndiponso tidzayamba kukondana kwambili . Zosoŵa za wolandila mphatso . M’bale Guy Pierce anali kukhulupilila kuti malonjezo a Yehova nthawi zonse amakwanilitsidwa mofanana ndi mmene timakhulupilila kuti dzuŵa lidzatuluka maŵa . ( 2 Timoteyo 3 : 16 ) Ndiye cifukwa cake tiyenela kuona Malemba onse kukhala ofunika kwambili pamene tiŵelenga Baibulo . ( Miy . 8 : 22 - 31 ) N’zoonekelatu kuti ngakhale asanabwele padziko lapansi , Yesu anali kukonda anthu . Koma Baibo imatitsimikizila kuti ngati ‘ timufunafuna Mulungu . . . tidzamupezadi . ’ Pa nyumba ina ya mzungu , tinali kutsuka mawindo . Popeza kuti msilikaliyo anali pafupi na pamene panali abalewo , iwo anamvela pamene bwana wakeyo anali kukamba kuti , “ Mungowatulutsa panja n’kukawawombela mfuti ! ” Komabe nkhani ino ingatitonthoze . Daniel anati : “ Tinali kufuna kulila tikaganizila zobwelela kwathu ku Spain . N’cifukwa ciani tifunika kucita zonse zotheka kuti tikapezeke pa Cikumbutso ? N’cifukwa ciani nthawi zina zingakhale zovuta kuonetsa cifundo ? Pamenepa , Mulungu anaonetsa cisomo cake . ” Nanga n’cifukwa ciani n’lofunika kwambili ? Koma Yehova amaona atumiki ake onse kukhala ‘ ofunika , ’ kuphatikizapo ao amene amaoneka ngati ofooka . Ndinakhala katswili pankhani yakuba . Ndinali kukhalapo amai akamaphunzila , ndipo ndinali kukondwela ndi phunzilolo . 1 - 3 . ( a ) Ndi mavuto ati a zacuma amene ena amakhala nao ? Nanga amacita ciani pofuna kuwathetsa ? ( 1 Akorinto 13 : 4 - 8 ) Ngati tisinkhasinkha mau a Paulo amenewa ndi kuwagwilitsila nchito , tidzakhala ndi banja lacimwemwe . Uthenga wake unali kudzagaŵanitsa anthu . 5 : 1 , 2 ) ‘ Timayenda m’cikondi ’ mwa kuonetsa khalidwe limeneli m’mbali zonse za moyo wathu . ( Yes . 54 : 13 ) Mpingo ndi malo abwino amene timapezamo citetezo ndi citsogozo cifukwa ndi kumene akulu amapeleka thandizo ndi uphungu wa m’Malemba . ( Agal . Conco kukhala na zimasulilo zatsopano za Baibo n’kothandiza kwambili . Odala ndi anthu onse amene amamuyembekezela . ” — Yes . Iye anapatsa Adamu na Hava zinthu zonse zofunikila kuti akhale na cimwemwe , komanso kuti akhale na ufulu weni - weni . Ngakhale ana amasangalala kwambili akadziŵa kuti makolo ao amawakonda . Ponena za thandizo limene iye ndi alongo ena osakwatila analandila , mlongo wina amene wakhala mu utumiki wanthawi zonse kwa zaka pafupifupi 50 , anati : “ Pakapita miyezi ingapo , akulu a mpingo wathu anali kuwacezela apainiya . Kodi Abisai anaonetsa bwanji kuti anali wokhulupilika kwa Davide ? ( Onani ndime 16 , 17 ) Kapena angasonkhezele anzathu kunchito kapena kusukulu kuti azitiseka cifukwa cotsatila makhalidwe abwino a m’Baibo . Kuonetsa Kukoma Mtima Kamodzi Cabe , Oct . ( 1 Sam . 17 : 34 , 35 ) Anaonetsanso kulimba mtima kwambili pamene anamenyana ndi ciphona codziŵa bwino nkhondo . Ndi zinthu zina ziti zimene zathandiza kuti nchito yolalikila padziko lapansi itheke ? Iye anati : “ Inu akazi , muzigonjela amuna anu , pakuti zimenezi ndiye zoyenela kwa anthu otsatila Ambuye . mu Galamukani ! 19 : 29 ) Yesu anati ophunzila ake adzalandila madalitso oposa zimene anasiya kaamba ka Ufumu . Tinalalikila nyumba zonse za kum’mwela ca kum’mawa kwa Irish Republic , popanda covuta ciliconse . Ndiyeno , tinali kuyamba kukambilana naye za Mlengi . Polimbana ndi mavuto , dalilani Yehova , ndipo citani zabwino Amayamba kukumana kaŵilikaŵili ndi kumanamizila kuti amangokumana mwangozi . Kodi Yehova watipatsa mautumiki ati ? Ndinakwatilanso Carmen mkazi wanga wokongola , ndipo tikukondwela m’cikwati cathu . Iye anati : “ N’nayamba kuseŵenzetsa mfundo za m’Baibo mu umoyo wanga . Zotulukapo zinali zakuti , ine ndi a m’banja langa tinayamba kulemekezana . ” Tiyenela kum’konda ndi mtima wonse ndi kum’tumikila ndi mtima wathu wonse , maganizo athu onse ndi mphamvu zathu zonse . Anali kuika zinthu zauzimu patsogolo . Popeza n’nali kuona zithunzi zambili zamalisece , n’nayamba kuzikonda . Pambuyo pa zaka zoposa 60 , mtumwi Yohane analemba kuti : “ Yesu anali kukonda . . . Zinthu zinasintha pamene cisumbali canga caciŵili cinayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . Kenako Yosefe anagwelamo . Conco , iye anati : “ Nditungilanso madzi ngamila zanu mpaka zitamwa mokwanila . ” — Genesis 24 : 17 - 19 . Kristu anacilikiza ulamulilo wa Yehova wacilungamo ndipo anaonetsa kuti anthu angwilo angakhale okhulupilika ngakhale akumane ndi mayeselo otani . Izi zidzacititsa anthu amene amafuna kukhala amtendele kubwela mumpingo wacikhristu . Kodi tingatsatile bwanji citsanzo ca Yehosafati ? M’malo mwake , vimacita nchito zoipa kuti cifuno ca Mulungu cisakwanilitsike . Vutoli limakhudza Akristu onse . 25 : 34 . Tisaleke kusonkhana pamodzi , monga mmene ena acizoloŵezi cosafika pamisonkhano akucitila . Koma tiyeni tilimbikitsane , ndipo tiwonjezele kucita zimenezi , makamaka pamene mukuona kuti tsikulo likuyandikila . ” Cifukwa ca khalidwe lao loipa , Akristu ambili a ku Korinto anali ‘ ofooka ndi odwaladwala , ndipo angapo anagona mu imfa [ ya kuuzimu ] . ’ Izi zionetsa kuti iye amawakonda kwambili anthu . N’ciani cingatilepheletse kutsatila malangizo a Yehova ? Koposa zonse , cifukwa cokonda Yehova ndi kumvela malamulo ake , iye amatithandiza ndi mzimu wake umene ndi wamphamvu kuposa cina ciliconse m’cilengedwe . Amalasa munthu mumtima mpaka kulekanitsa moyo ndi mzimu , komanso mfundo za mafupa ndi mafuta a m’mafupa . Mawu a Mulungu amathanso kuzindikila zimene munthu akuganiza komanso zolinga za mtima wake . ” Mwacitsanzo , pamene Davide analemba Salimo 55 , anali kudela nkhawa moyo wake . ( Sal . Koma sikuti Paulo anali kulalikila cifukwa coopa mlandu wa magazi kapena cifukwa congofuna kukwanilitsa udindo wake ayi . Mwacitsanzo , Yehova anakamba mau aulosi amene analimbikitsa Ayuda amene anali mu ukapolo ku Babulo . Akhiristu Anzathu ndi anthu amene angatitonthoze tikakumana na mavuto . Tikakhala pa misonkhano , timaphunzila Mau a Mulungu na kulimbikitsana . Izi zimatithandiza kuikabe maganizo athu pa mphoto . 18 : 35 ) Yesu anafotokoza zimenezi atangopeleka pemphelo lacitsanzo . Ndipo wopusa kwambili ndi munthu amene amakhulupilila zimene waŵelenga cifukwa cakuti zalembedwa m’nyuzipepala . ” — Anatelo August von Schlözer , wolemba mabuku ndi mbili yakale wa ku Germany ( 1735 - 1809 ) . Afunika kulekelatu kucita macimo , osati mwa kupewa cabe macimo aakulu , komanso ngakhale zolakwa zina zazing’ono zimene kaŵili - kaŵili zimatsogolela ku chimo lalikulu . ( Aef . 5 : 1 ) N’zoona kuti anthufe tinalengedwa kuti tizicitila ena cifundo . ( 1 Maf . 3 : 12 ; 11 : 1 , 2 ) M’Cilamulo ca Mulungu , munali lamulo lacindunji loletsa mfumu ya Isiraeli ‘ kudziculukitsila akazi kuti mtima wake ungapatuke . ’ ( Deut . Helens , ku Tasmania Tiyeni tione mmene Mulungu wawadalitsila . 24 : 14 ) “ Mzimu ndi mkwatibwi akunenabe kuti : ‘ Bwela ! ’ ” 13 : 20 ) Zidzakhaladi zosangalatsa kupulumuka mapeto a dongosolo loipali ndi kukhala m’dziko latsopano la Yehova . ( Afil . 1 : 7 ) Ndipo pamene oweluza a ku makhotiwo anali kufuna kutilanda ufulu wathu wolalikila , tinacita apilo ku makhoti apamwamba ndipo nthawi zambili tinapambana milanduyo . 20 : 12 , 13 ) Dziko lonse lapansi lidzakhala paladaiso monga mmene munda wa Edeni unalili . 23 Pitani Patsogolo Monga Munthu Wauzimu Pamene nkhondoyi inali kutha m’caka ca 1918 , padziko lonse panagwa njala yadzaoneni ndi mlili wa fuluwenza umene unapulula anthu ambili kuposa amene anafa pa nkhondo . Nanga anakwanitsa bwanji kuthandiza anthu wamba kumvetsetsa Mau a Mulungu ? ( b ) Ndani amene afunika kuimbidwa mlandu ngati munthu wagonja pa ciyeso ? Kodi munatambako filimu imene kwa inu , zinali zocita kuonekelatu kuti munthu wina akumunyengelela mpaka kumusoceletsa ? Cikondi ceniceni sicikwiya msanga , ndipo “ sicisunga zifukwa . ” Sitiyenela kucita ngati tikulemba zolakwa za ena m’buku . Mmene Tingakhalilebe ndi Maganizo Oyenela , 3 / 1 Nthawi zingapo pamene iye anafooka , anaona kuti ndiye anali mapeto a moyo wake . Kodi anthu a fuko la Rubeni , Dani , ndi Aseri anasiyana bwanji ndi a fuko la Zebuloni ndi la Nafitali ? Anadalila Yehova . Mudzakhala “ Ufumu wa Ansembe , ” 10 / 15 Timasangalala kuti Yehova mwacisomo cake , walola kuti anthu amitundu yosiyana - siyana amvele uthenga wabwino . 4 Kodi Amuna Anayi Okwela pa Mahosi N’ndani ? M’banja lathu tinabadwa ana aamuna anayi , ndipo ine ndine waciŵili . M’bale Charles Taze Russell ndi anzake anacita khama kuti apeze coonadi ca m’Baibulo ndi kutumikila Yehova . Mumaphunzilanso kugwila nchito pamodzi na Yehova . — 1 Akor . Paulo analimbikitsa Akristu onse kuti ‘ aziganizila ’ zofuna za okhulupilila anzawo . Inde , ngakhale pamene tinali m’ndende , kukhulupilika kwathu kunacititsa anthu ena kutamanda Yehova . 10 Thandizo pa Kuthetsa Mavuto Ndinafooka mwakuuzimu . ” ( Miy . 16 : 20 ) Baruki , mlembi wa Yeremiya , anaiŵala mfundo imeneyi . Tingaonetse bwanji kuti timayamikila mwai wodziŵika ndi dzina la Mulungu ? KATHERINE anakulila ku United States , ndipo anabatizika monga Mboni ya Yehova ali ndi zaka 16 . Nanga Mau a Yehova amatilimbikitsa kucita ciani ? — Ŵelengani Mlaliki 12 : 1 . Conco , tikulimbikitsidwa kuti nthawi ikakwana , tizikhala pansi na kumvetsela mwachelu nyimbozi . Titabwelela ku Malawi , ndinauzidwa kuti ndikacezele mipingo mumzinda wa Lilongwe , umene ndi likulu la dzikoli . Kuyankha mwacidule , cifukwa cinali cakuti zinthu zinali zovuta ngako nthawi imeneyo . Timalalikila pofuna kucenjeza anthu . Usiku umene Yesu anayambitsa Cikumbutso , anaona kuti atumwi ake anali atayamba kudzikuza . Kumeneko kunali kusonkhana Mboni zacikulile 12 . Koma zoona n’zakuti anthu amene anabadwa tsiku limodzi - modzi sakhala na makhalidwe ofanana . Deti la kubadwa la munthu silionetsa ciliconse cokhudza khalidwe limene adzakhala nalo . ( Gen . 39 : 1 - 12 ; 41 : 38 - 43 ) Akristu ayenela kupewa kugwela m’chimo ndi munthu amene si mwamuna kapena mkazi wao kaya ali kunchito kapena ku malo ena obisika . Zimakhala conco cifukwa pounyula , mumacotsa ina mwa mizu yake kuti usakuvuteni kunyamula . DZIKO : LEBANON Tingaonetse kuti tilidi na cikondi ceni - ceni ngati titsatila lamulo la m’Baibo lakuti “ thandizani ofooka , khalani oleza mtima kwa onse . ” Anthu amene adzaukitsidwa adzakhala na ciyembekezo cokhala na moyo wangwilo kwamuyaya . Mosakaikila , mudzalimbikitsidwanso kukhala woolowa manja kwambili , wacikondi , ndi wokonzeka kukhululukila ena . ( Akol . 3 : 13 ) Komabe , banja lingaonongeke ngati okwatilana amakumbutsana zolakwa zakale akakhumudwitsana . Koma patapita nthawi anayamba kulakalaka kuti anthu azimulambila . Ngati akulu amanyalanyaza kuphunzitsa ena , m’kupita kwa nthawi mumpingo mungasowe abale oyenelela amene angasamalile maudindo . Yaciŵili , popeleka yankho lake , Yesu anachula Abulahamu , Isaki , ndi Yakobo , amene anali makolo okhulupilika amene adzaukitsidwa kudzakhala ndi moyo padziko lapansi . — Luka 20 : 37 , 38 . Ngati ndi kotheka , khalani mwamtendele ndi anthu onse , monga mmene mungathele . . . . Yehova amafuna kuti tizipemphela kucokela mumtima . Pamene Filipo anauza Natanayeli kuti wapeza Mesiya , Natanayeli anati : “ Kodi mu Nazareti mungatuluke kanthu kabwino ? ” 3 Funso Logometsa Mutu Zaka za m’ma 500 C.E . mpaka 1500 C.E . : Abusa ena Acikatolika anali kukwiya kwambili akaona mamembala awo ena akulalikila zimene Baibulo imaphunzitsa , m’malo mwa ziphunzitso za Cikatolika . Sitidabwa ngati anthu a m’dzikoli aticitila zinthu zankhanza . M’malo mwakupha opandukawo nthawi imeneyo , Mlengi wanzelu anakhazikitsa pangano la mu Edeni . Anacita zimenezi kuti mau ake akwanilitsike . — Ŵelengani Genesis 3 : 15 . Kuyambila nthawiyo , iye anaonetsa cikondi cake pa Khristu mwa kugwila mwakhama nchito yopanga ophunzila , ndipo anakhala mzati mumpingo wacikhristu wa m’zaka 100 zoyambilila . Mwa kuona kwa umunthu , ampatuko amenewa anali ofanana ndi ena onse mu mpingo . ( b ) Mogwilizana ndi Miyambo 15 : 22 , n’cifukwa ciani tifunika kukambilana malangizo amene abale ena anapeleka ? Makenzie , wa zaka 23 , anati : “ Ngati anzako umacita nawo zinthu mokoma mtima na kuwamvetsela mwaubwenzi , umadziŵa zovuta zimene akukumana nazo . Nkhani yokamba za cilengedwe m’buku la Genesis limati : “ Yehova Mulungu anaumba munthu kucokela kufumbi lapansi , ndipo anauzila mpweya wa moyo m’mphuno mwake , munthuyo n’kukhala wamoyo . ” Coyamba , tiyenela kukhala ofunitsitsa kupatula nthawi yophunzila ndi kusinkhasinkha zimene Yesu anakamba , kufufuza ndi kufunsa mafunso oyenelela . Pokamba za mmene zikwangwani zinathandizila polengeza za msonkhanowo ku Mexico City , magazini yochedwa La Nación inati : “ Tsiku loyamba [ la msonkhano wadela , Mboni ] zinauzidwa kuti ziitanile anthu ambili . Ngakhale kuti tingadzikaikile , Yehova angatithandize kucita zinthu zimene sitinaganizilepo kuti tingakwanitse . Angelo anathandiza amuna oimilako Mulungu . Yesu anasankhidwadi ndi Yehova . 52 : 7 ; Aroma 10 : 15 ) Ngakhale n’conco , Mkhristu amafunika kulimba mtima kuti alalikile pamene mpata wapezeka . Mlongo wina amene anatonthozedwa ndi Akristu anzake mwana wake wa mkazi atamwalila anati : “ Ndinali kuyamikila kwambili pamene anzanga ena anali kubwela kudzangolila nane basi . ” Mwacitsanzo , ang’ono anga aŵili anasiya coonadi . Lumbilo limeneli ni nkhani yaikulu . Yehova ndi wofunitsitsa kukuthandizani monga mmene wathandizilanso abale anu ambili kupeza ciyanjo ndi madalitso a Mulungu , ngakhale kuti ndi opanda ungwilo . [ Cithunzi papeji 10 ] Kodi Petulo anacitanji atadzudzulidwa ? Kodi ifenso tingacite mofanana ndi iye ? ( Onani ndime 15 ) Andebele ndi ocepa ku South Africa , ali cabe ciŵelengelo ca 2 pelesenti Yesu anaonetsa kuti anthu afunika thandizo kuti amvetsetse zimene iye anali kuphunzitsa . Patapita miyezi 6 , n’nayamba upainiya wothandiza . Iye anavutika cifukwa cotaikilidwa mwamuna wake , ndipo anapondelezedwa ndi atsogoleli acipembedzo amene anali ‘ kudyelela nyumba za akazi amasiye ’ m’malo mowathandiza . Pa nthawi imeneyo , abale osakwatila pafupi - fupi 12 ndiwo anali kutumikila kumeneko . Mtundu wina wa codzitetezela pa cifuwa cimene asilikali aciroma anali kuvala m’nthawi ya atumwi , cinali kukhala na tunsimbi topyapyala toikidwa mosanjikiza . Pamene anayamba kulamulila , mwacionekele Rehobowamu anazindikila kuti Aisiraeli sanali okondwela . * Mofananamo , pofotokoza fanizo la matalente , Yesu sanali kutanthauza kuti odzozedwa ambili m’masiku otsiliza adzakhala oipa ndi aulesi . Koma zimenezi sizitanthauza kuti Mau a Mulungu amaletsa kukhala ndi malo abwino kuti mupemphele , muphunzile , ndi kusinkhasinkha . Tangoganizilani nili wam’ng’ono n’tanyamula cigilamafoni ! Nkhanza zimene zilipo masiku ano pa dziko lapansi zidzathelatu pa “ tsiku laciweluzo ndi ciwonongeko ca anthu osaopa Mulungu . ” Azimai amenewa atabwelanso , anandipempha kuti ndiziphunzila nao Baibulo , ndipo ndinavomela . 18 : 1 ; Aheb . 3 : 12 , 13 ) Mkristu wokhwima mwauzimu angatithandizenso kudziŵa zinthu zoipa zimene tiyenela kusintha pa umoyo wathu kuti tikhalebe m’cikondi ca Yehova . Akulu ndi atumiki othandiza analimbikitsidwa ‘ kuweta nkhosa za Mulungu zimene anazisiya m’manja mwao . ’ Patapita nthawi yocepa , Dennis anatumiziwa ku Ireland . Conco , Arthur anatsala yekha . Anthu ena anali atacitapo kale zimenezi . Adzangoiŵalako zolakwa zanga . ’ Samueli atangoleka kuyamwa , mwina ali na zaka zitatu , Hana anacita ndendende zimene analonjeza Mulungu . ( Maliko 10 : 29 , 30 ) Komanso , awo amene amacita khama kufuna - funa Mulungu , amalandila madalitso osaneneka , monga mtendele wa maganizo , kukhala okhutila , na cimwemwe . — Afil . Kodi goli la Yesu n’lofewa m’lingalilo liti ? Ndipo kudziŵa zimenezi kuyenela kutikhudza bwanji ? ( Luka 22 : 29 , 30 ; Chiv . 5 : 10 ; 7 : 4 - 8 ) Mofananamo , Yesu analamula otsatila ake ocepa , omwe anamuona ataukitsidwa , kuti ayenela kulalikila . ( Mac . Nthawi yabwino yocita zimenezi m’pamene muceza . Ngakhale pamene Yesu anali kumva ululu wosaneneka pamtengo wozunzikilapo , anapemphela kwa Atate ŵake kuti awakhululukile aja amene anamupha . Iye anati cifukwa “ sakudziŵa cimene akucita . ” Samuelson ) , Mar . 22 Mulungu “ Akwanilitse Zofuna Zanu ” Tiphunzilapo ciani pa nsembe zimene Aisiraeli akale anali kupeleka ? Akulu ayenela kukupemphani fon’namba imene angaseŵenzetse pakagwa tsoka kuti adziŵe za inu . Pa cifukwa cimeneci , Yehova anamudalitsa mwa kumuukitsa ndi kumuika kukhala Mfumu ya Ufumu wakumwamba . — Mateyu 28 : 7 , 18 - 20 . ▪ Kuthandiza Abale a Kristu Mokhulupilika Conco , ayenela kuti anadziŵa kuti colengedwa camzimu n’cimene cinakamba na Hava kupitila mwa njoka . ( Gen . N’zoona kuti anthu ambili samvetsela uthenga wathu . Paulo anacita kukamba kanayi kuti “ ena mwa iwo ” sanamvele . Atatitengela mafaelo , tinada nkhaŵa cifukwa munali makalata ambili ofunika . Dzina lakuti Satana limachulidwa maulendo 18 cabe m’Malemba Aciheberi . Koma m’Malemba Acigiriki Acikhristu limachulidwa koposa ka 30 . Ndiyeno mu 2013 , ofesi ya nthambi ya ku Puerto Rico anaiphatikiza ndi ya ku United States , ndipo ine ananitumiza ku ofesi ya nthambi ya ku Wallkill , ku New York . Ndiponso Yehova analenga thupi la munthu m’njila yakuti lizitha kudzicilitsa . Munthu wokhumudwa amasokoneza mzimu wa mpingo . Muzicita zimene mungathe kuti muphunzitse ana anu Mau a Mulungu mowafika pamtima . Ganizilani zimene Yonatani anacita Sauli atangoyamba kupandukila Mulungu . Ndipo mipingo potsatila malamulo amenewo , “ inapitiliza kulimba m’cikhulupililo ndipo ciŵelengelo cinapitiliza kuwonjezeka tsiku ndi tsiku . ” ( 2 Mbiri 17 : 3 - 10 ) Ngakhale kuti Yehosafati anacita zinthu mopanda nzelu , Yehova sanaiŵale zabwino zimene anacita poyamba . Koma Aisiraeli anali kupatsa Aleviwo cakhumi , cimene cinali kuwathandiza kuti aziika mtima wawo pa nchito yawo ya pa cihema . ( 1 Sam . 9 : 21 ) Iye anakana kulanga Aisiraeli amene ananyoza ulamulilo wake , ngakhale kuti kunali koyenela kucita zimenezo kuti ateteze udindo wopatsidwa ndi Mulungu . 6 , 7 . ( a ) Fotokozani udindo umene akulu anali nawo poweluza munthu wopha mnzake mwangozi . Zimene anapeza ataiphunzila , zinam’cititsa cidwi . Mungacite ciani kuti mupewe zimenezi ? Mzimu woyela umalimbikitsanso Akhiristu odziŵa zambili kuti athandize anthu amene afuna kumvetsetsa Baibo . — Machitidwe 8 : 26 - 35 . Kodi mphatso imeneyi imatilimbikitsa kucita ciani ? Mkati mwa masiku ano otsiliza , magulu onse aŵili amagwilila nchito pamodzi yopanga ophunzila mwacangu monga “ gulu limodzi . ” — Yoh . 10 : 16 . Ena amalandila uphungu cifukwa cakuti akungofunikila kutelo . ( a ) Kodi pali pano tingauthetse mtima wodzikonda ? Conco , pokhala ndi cakudya , zovala ndi pogona , tikhale okhutila ndi zinthu zimenezi . ” Koma muyenela kukumbukila kuti Khristu anamufela munthuyo , ndipo inu mufunika kumukonda . Munthu amapeza cimwemwe ceni - ceni komanso cokhalitsa ngati acita cifunilo ca Mulungu , na kudziŵa kuti akukondweletsa Yehova . Ngati sitingawauze , ena angayambe kugwilizana nafe cifukwa cofuna cabe thandizo lakuthupi . ” Iye anakamba kuti : “ Pamene mlongoyo ananiuza mmene moni wanga wacidule unamukhudzila , n’nakondwela kuti n’namupatsa moni . ( Miyambo 22 : 29 ) Mwina munthu wina angakuuzeni kuti mankhwala ocilitsa matendawo apezeka kwinakwake kutali , koma madokotala akalibe kuwadziŵa . Mofananamo , mphunzitsi amafunika kukonzekeletsa mtima wa wophunzila asanayambe kumuphunzitsa zinthu zatsopano . Kodi tingaphunzilepo ciani pa zitsanzo za anthu auzimu ? Lomba nili na zolinga zatsopano pa umoyo . ” — Raquel Iye ndi mkazi wake Maureen , anakamba kuti cinthu cimodzi cimene asangalala naco kwambili ku Warwick ndi “ kukumana ndiponso kugwila nchito ndi abale ndi alongo ambili amene adzipeleka kutumikila Yehova pa Beteli kwa zaka zambili . ” 13 , 14 . ( a ) Pangano latsopano ndi logwilizana motani ndi Ufumu ? Kodi Mike ndi banja lake anacita ciani ? ( Mateyu 22 : ​ 35 - 37 ) Pamenepa , Yesu anasonyeza kuti munthu ayenela kubatizidwa ndi kukhala Mkristu cifukwa cokonda Yehova . 141 : 5 ; Miy . Davide anauza mfumu mau olimbikitsa ponena za Goliyati . Iye anati : “ Musalole kuti aliyense agwidwe ndi mantha mumtima mwake . ” Maganizo amenewo anacititsa kuti ndiyambe kumva cisoni kwambili ndi kudziimba mlandu . Koma pambuyo pake , “ Hezekiya anadzicepetsa , ” ndipo mkwiyo wa Mulungu sunamugwele iye pamodzi ndi anthu ake . — 2 Mbiri 32 : 25 - 27 ; Sal . 20 : 35 ; Afil . Ndiyeno , Eliya anauza Ahabu kuti Yehova adzathetsa cilala ndipo adzagwetsa cimvula . Ngati timamvela Yehova , iye adzaonetsa kuti amatikonda . Anthu ambili sadziŵa kuti zinthu zimene timafunikila zisiyana ndi zimene timalakalaka . 17 : 3 , 11 . Marita anali wotsimikizila za ciukililo cifukwa ayenela kuti anamvapo za anthu amene anaukitsidwa Yesu asanayambe ulaliki wake . Popeza tikali “ m’nthawi ” yovuta , tidzapitiliza kukumana na mavuto amene adzayesa kukhulupilika kwathu kwa Yehova . Komabe , ngati sitisamala , tingaleke kuyamikila cuma cimeneci , mpaka kufika pocitaya , titelo kunena kwake . Anatsimikiza mtima kumvela “ Mulungu monga wolamulila , osati anthu . ” ( Mac . Wosimba ni Beishenbai Berdibaev Muziona aphunzitsi anu ngati bwenzi lanu ndipo muzionetsa kuti mumayamikila kuyesayesa kwao pokuthandizani . Ndipo iye lomba akupatsa mwana wake Solomo mapulaniwo . 32 : 1 , 2 ) Ganizilani mmene timakhalila otetezeka ku cimphepo camphamvu , ku mvula yamkuntho kapena mmene timamvelela tikakhala pamthunzi kukatentha kwambili . Yesu anakamba kuti anthu ena “ adzaona Mulungu . ” Kulimbikitsa anthu kupita pa webusaiti ya jw.org kumathandizila polengeza “ uthenga wabwino . ” Ngakhale n’conco , uthenga umene timalalikila udzatithandiza kuti tidzapeze moyo wosatha pamodzi ndi anthu amene amamvetsela uthengawo . Linda anali kuopa kupita muulaliki akaganizila zimene ena angaganize ndi kukamba akamuona . Tiziphunzila ndi kugwilitsila nchito Mau a Mulungu nthawi zonse . Kodi maganizo abwino angatithandize bwanji ? Monga mmene taphunzilila , maganizo abwino angatithandize kutsanzila makhalidwe a Yehova monga cikondi . ( 1 Tim . 2 : 14 ; 5 : 11 ) Akristu a ku Tesalonika amenewa anapilila cizunzo cifukwa anali kugwilizana kwambili , kukondana , ndi kuthandizana . Iye akulephela kupuma bwinobwino , ndipo akusowa cocita . Koma popeza kuti ndikudziŵa cifukwa cake , ndi kuti Mulungu adzathetsa nkhanza posacedwapa , mtima wanga umakhala pa mtendele ndipo ndimakondwela kwambili . — Salimo 37 : 29 . [ Mau okopa papeji 9 ] Njila yabwino koposa imene io angathandizile abale a Yesu ndi mwa kugwila nao nchito yolalikila . Kodi Toñi anacitanji ? Motelo pakubuka funso lakuti : N’cifukwa ciani lemba la Yeremiya 31 : 15 limanena kuti iye anali kulila cifukwa ana ake “ kulibenso ” ? Conco , ayenela kuti anali na katundu wambili . ( Akol . 1 : 10 ) Komabe , kukhala na cidziŵitso pakokha si kokwanila . 110 : 1 . 11 : ​ 5 , 6 , 10 ) Koma ngati afuna , angapemphe m’bale wobatizidwa kuti acititse phunzilo limenelo ngati m’baleyo ndi woyenelela . Koma tingapindule ngati timaganizila zimene iye anacita kuti atikhululukile . Kodi si zimene tingayembekezele kwa Mulungu amene amalemekeza ufulu wathu , komanso amene nthawi zonse amaonetsa makhalidwe ake mwacikondi ? — Deut . 20 Tengelani Citsanzo ca Atumiki Okhulupilika a Yehova N’nabatizika mu March 1957 . Apa n’kuti papita miyezi 9 cabe kucokela pamene n’napezeka pa phunzilo ya buku ija . Mwacitsanzo , Sitefano anafa ali ndi cikhulupililo cakuti akufa adzauka . — Mac . 7 : 55 - 60 . Angacite zimenezo mwa kuika Yehova Mulungu ndi Ufumu wake patsogolo mu umoyo wao . NYIMBO : 127 , 88 Nyimboyo inanigwila mtima kwambili , ndipo n’naganiza zokhala . TSAMBA 12 • NYIMBO : 108 , 24 Masiku ano , pali matenda ena amene alibe mankhwala . Tangoganizilani mmene Yehova na Yesu adzakondwelela popenyelela anthu mamiliyoni pa dziko lapansi , akusonkhana pa cocitika cimeneci , ola ndi ola mpaka kutha kwa tsikulo . Koma m’kupita kwa nthawi Fernando anayamba kukaikila ngati adzayenelela kukhala mkulu . Kumbali ina , anali na nkhawa yakuti anthuwo akhoza kum’pandukila akakana pempho lawo . Ponena za nyenyezi , nyuzipepala ina ya ku Houston , m’cigawo ca Texas , inafotokoza kuti kafukufuku waposacedwapa anaonetsa kuti pali nyenyezi zokwanila “ 300 sekisitiliyoni , kapena kuti kuwilikiza katatu kuyelekezela ndi ciŵelengelo cimene asayansi anapeza m’mbuyomu . ” Iwo anamuuza kuti : “ Thawani mupulumutse moyo wanu ! ” ( Gen . Za conco zikacitika , mwina mumadzifunsa mmene mungalangile mwana wanu , ndiponso ngati ndi koyenela kupeleka cilango kwa mwanayo . Monga mmene mutu wankhani ukuonetsela , “ kulambila kwa pabanja ” ndi mbali imodzi ya kulambila kwathu Yehova . Ni madalitso anji amene timapeza ngati tinadzipeleka kwa Yehova ? Kodi zifooko za amuna oimila Mulungu zinacititsa Aisiraeli kuti asatsatile citsogozo cawo ? ( 1 Akor . 7 : 39 ) Akaloŵa m’banja , nawonso amadzavomeleza kuti Baibulo ndiyo imapeleka uphungu wabwino kuposa munthu aliyense , kuti banja lipambane . Popeza n’zosatheka kudziŵa maina a odzozedwa onse amene ali padziko lapansi , zingatheke bwanji ‘ kupita nao limodzi ’ ? Imapeleka malangizo othandiza pa nkhani izi : M’CAKA ca 1970 , ndinagonekedwa m’cipatala cina m’dela la Phoenixville ku Pennsylvania , m’dziko la United States cifukwa codwala matenda ena ake oopsa . ▪ Makolo — Ŵetani Ana Anu Ngati ni yongolota , n’cifukwa ciani anthu amacita nayo cidwi ? Koma izi sizitanthauza kuti tifunika kutengela ndendende ciliconse cimene mkulu winawake amacita , monga kakambidwe kake ka nkhani , kavalidwe kake , mmene amadzikonzela , kapena mmene amakambila ndi anthu . Imfa ya Yesu inacitikadi , ndipo inatsegula njila yodzakhala ndi moyo kwamuyaya . Koma tikasiya , tingagonje kwa Satana , dziko lake , na zofooka zathu . Kuti tate amene alela ana ndi kusamalila banja ayende na Mulungu , afunika kusamalilanso banjalo pa zinthu zauzimu . N’nali kumvela monga nkhawa zikunimeza wamoyo . ” 25 : 31 - 33 ; Mac . 20 : 35 . 3 : 18 , 19 ; Yuda 4 , 8 , 12 ) Kumbukilaninso m’bale wa ku Korinto uja amene ‘ anatengana ndi mkazi wa bambo ake . ’ Kodi zotsatilapo zake zakhala zotani ? Muzicita zoposa zimene mwauzidwa kucita . Tikali kukhala m’nthawi imeneyi , ndipo mapeto a dongosolo lino la zinthu ali pafupi kwambili . Baibo ya Septuagint inathandiza kwambili Ayuda ndi anthu ena amene anali kukamba Cigiriki kuti azitha kuŵelenga Malemba amene poyamba anali m’Ciheberi . Baibulo silionetsa utali wa nthawi imene Rabeka anakhala ku citsime . Dziko likuonongedwanso m’njila ina . Mungawathandizenso kukhala alaliki ogwila mtima mwa kuwauzako zokhudza mbili ya delalo , kapena kuwafotokozela zikhulupililo za cipembedzo zofala m’delalo . Ngati timaganizila mmene zocita zathu zingakhudzile ubwenzi wathu ndi Yehova , komanso ngati timatsatila miyezo yake posankha zinthu , ndiye kuti tayamba kupeza nzelu zopindulitsa . ( Yobu 28 : 28 ) Kuti Yehova athandize Mose kukhala ndi mantha ndi kucita zinthu mwanzelu , anamuonetsa kusiyana kumene kulipo pakati pa anthu ndi Mulungu Wamphamvuyonse . N’zoona kuti Yehova samadalila thandizo lathu kuti akwanilitse cifunilo cake . Acikulile ena amakhala ndi thanzi la bwinoko ndipo sakhala ndi vuto loiŵalaiŵala . Anadziŵa kuti akamvela anthu , iye , banja lake , ndi a m’nyumba yacifumu adzafunika kudzimana zinthu zina zimene anali kukonda , ndipo sakanakhala na ufulu wongolamula anthu zimene akufuna . 3 Yehova Anamucha kuti “ Bwenzi Langa ” Ngati tifufuza mosamalitsa , tingapeze mfundo zabwino za m’Mau a Mulungu . Michael anakamba kuti anayambitsa maphunzilo atatu ndipo afuna thandizo powaphunzitsa . ” Ganizilani zimene munacitila Yehova mu utumiki caka catha . Conco mu 2002 , iye anasamukila ku Russia . Masiku ano , Nsanja ya Mlonda imasindikizidwa m’zinenelo zoposa 200 . ( Yohane 14 : 26 ) Conco , Mulungu amapeleka mzimu woyela , mphamvu yake yogwila nchito , kuti uthandize anthu kumvetsetsa zimene amaŵelenga m’Baibo . Ena analeledwa ndi makolo amene anawaphunzitsa mfundo za m’Baibulo . ( Deut . Mofananamo , akulu amatithandiza ndi kutilimbikitsa kuti tipitilizebe kutumikila Yehova ngakhale kuti timakumana ndi mavuto . N’zomveka kuti mau amenewo anali kumukhumudwitsa Zoila . N’zosavuta kudziŵa cifukwa cake sanafune kukhala wosauka kwambili . Mwacionekele , akatswili ena anali atafalitsapo kale Baibo ya Cipangano Catsopano yomasulidwa m’Ciheberi . Baibo imakamba za Mlengi wathu , Yehova Mulungu , kuti : “ Inu ndinu kasupe wa moyo . ” Tingakonzekele bwanji kudzakhala ndi moyo m’dziko latsopano ? M’malomwake , timayesetsa kukhala odzipeleka kaamba ka Ufumu wa Mulungu . ( Mat . Anthu ena angationetse tsankho kapena ise tingakhale nalo khalidwe limeneli . Koma Naboti anali kuona kuti ubale wake na Yehova ni wa mtengo wapatali kuposa ngakhale moyo wake . Conco , muziyesetsa kupeza nthawi yoŵelenga ndi kuphunzila zinthu zatsopano . Mau amene Paulo analembela Akhristu a ku Filipi aonetsa kuti cimene cingacepetse nkhawa ni pemphelo . Atumiki a Yehova amaphunzila coonadi m’njila zosiyana - siyana . Zimene Aisiraeli anacita zinali zolakwika kwambili . Panthawi imeneyo , ndinali nditangobatizidwa monga mmodzi wa Mboni za Yehova . Njila zimenezi zili m’munsimu . 55 : 11 ) Iwo anapatsidwa cilango ca imfa ndipo zotsatilapo za uchimo zinayamba nthawi imeneyo . Koma Mulungu analola Adamu ndi Hava kubeleka ana amene anali kudzapindula ndi makonzedwe ena . Komabe , onani kuti Petulo anauza Akhristu anzake kuti “ muzicelezana . ” Ndinaleka kukoka fodya kuti ndikondweletse Yehova . ” Hana , mkazi wokondedwa wa Elikana , anakumana ndi vuto lalikulu . Kodi mwaona mmene makhalidwe abwino a anthu alowela pansi ? Ndipo mwanda umodzi kuculukitsa ndi mwanda umodzi timapeza 100 miliyoni . Cotelo , mfumu inaitanitsa Davide . — 1 Samueli 17 : 23 - 31 . Popeza kuti siticilikiza maboma a anthu , timakhala ndi cikumbumtima coyela pamene tikulalikila kuti Ufumu wa Mulungu ndi umene udzathetsa mavuto onse a anthu . Pambuyo pa miyezi inayi , n’napemphedwa kuti nikatumikile monga mpainiya wapadela mu Austria . 3 : 5 - 7 . Pofotokoza ulosi wake wonena za mapeto a dongosolo lino la zinthu , Yesu anati : “ M’badwo uwu sudzatha wonse kucoka kufikila zinthu zonsezi zitacitika . ” Tsiku lina , nili na zaka 7 , cina - cake coopsa cinanicitikila . Pambuyo pake , n’napempha ku kampani ya zamafoni ija kuti nikayambe kuseŵenza pambuyo pa mawiki 5 . Komanso kumbukilani kuti kuŵelenga Malemba kunamukhudza mtima Yosiya ndipo kunamulimbikitsa kucitapo kanthu . MUNTHU AMAFUNIKILA KUBATIZIKA KUTI AKAPULUMUKE Ni Yehova na Yesu cabe amene amakwanitsa kucita zimenezi . Ngakhale akuluakulu amafunsila uphungu kwa makolo ao . CAKA COBADWA : 1960 Paulo analimbikitsa Akhristu a m’nthawi ya atumwi ‘ kuyesetsa mwakhama kuti akhale okhwima mwauzimu . ’ ( Aheb . NKHANI YA PACIKUTO MUNGACITE CIANI KUTI MUPINDULE NA ZIMENE MUŴELENGA M’BAIBO ? Zimenezi zinaseŵenza kwa anthu ambili . Cinawathandizanso kudziŵa kuti anafunika dipo , kapena kuti nsembe yangwilo imene ikanacotselatu ucimo wao wonse . Ina anaipeza m’zipululu . Kodi Yesu na Afarisi anali kusiyana bwanji pa nkhani ya mmene anali kuonela ocimwa ? Ngakhale Yesu nayenso analimbikitsiwa na Atate wake . Kunena zoona , kuti munthu akhale wodzicepetsa afunika kukhala wolimba mtima . Kodi kunyada n’kutani ? Ngakhale n’conco , mu 2014 , Sylviana anagwilizana na Sylvie Ann , mpainiya wacitsikana wa mu mpingo mwawo , ndipo anakukila ku mudzi wina waung’ono umene uli pa mtunda wa makilomita 85 kucokela m’tauni yawo . Ataphunzila coonadi , analeka cizoloŵezi cimeneci . Yehova “ amafuna kuti anthu onse alape . ” Barizilai anazindikila kuti zinthu kwa iye zinasintha tsopano , ndipo anali wacikulile . Madokota anadziŵa kufunika koseŵenzetsa mfundo imeneyi pambuyo pa milili ya matenda a m’zaka za pakati pa 500 C.E . na 1500 C.E . Kodi izi zindiphunzitsa ciani ponena za Yehova ? Mau a Mulungu amakamba momveka bwino kuti Davide anakalamba na kumwalila . N’zoona kuti kulalikila uthenga wabwino kungakhale kovuta . Iye anati : “ Ngati mufuna kusangalala na utumiki , mungacite bwino kukatumikila mumpingo wa citundu cina . Mwacikondi , Mboni za Yehova zikuitanani kuti mukabwele ku Nyumba ya Ufumu imene ili kufupi ndi kwanu kuti mukaone nokha mtendele ndi mgwilizano weni - weni umene uli pakati pao . — Salimo 133 : 1 . [ Bokosi papeji 30 ] Kodi Coonadi Cilikodi ? Ni pa zocitika ziti pamene mungaonetse khalidwe la cifundo ? Kodi Yehova anadzidziŵikitsa bwanji kwa Mose ? N’zolimbikitsanso kudziŵa kuti Yehova sakondwela ndi kulambila kwa cinyengo . Mwamsanga , Farao anatuma anthu kuti akaitane Yosefe kundendeko . — Genesis 41 : 9 - 13 . N’ndani adzawapezela zakudya na kuwasamalila ? ( Aheberi 13 : 23 ) Koma patangopita zaka 5 , Akristu a ku Yudeya , makamaka amene anali kukhala mu Yerusalemu , anafunika kucoka m’madela ao mwamsanga . Ndiyeno , pakati pa usiku , mwadzidzidzi kunacitika civomezi cimene cinagwedeza ndendeyo na kucititsa kuti zitseko za ndendeyo zitseguke . Yehova Mulungu anathandizadi Yoswa pa zilizonse zimene anali kucita . Koma coyamba , tiyeni tione zoona zake . Kodi zimatitengela nthawi yaitali bwanji kuti tikhululukilane ? Gwilitsilani nchito zofalitsa zathu kuti mukonzekeletse mtima wanu kaamba ka Cikumbutso ( Onani ndime 9 ) Pofotokoza lamulo la makhalidwe abwino , Yesu anati : “ Zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inunso muwacitile zomwezo . ” Zimenezi zinakwiitsa Yehova kwambili . — 1 Sam . Mosiyana ndi Meriba woyamba uja , Meriba waciŵiliyu anali kufupi na ku Kadesi , osati ku Masa . ( Yesaya 11 : 9 ) Yehova adzacititsa kuti maganizo ndi matupi athu akhale angwilo . Kodi mfundo za m’fanizoli ndingazigwilitsile nchito bwanji paumoyo wanga ? Ngati n’conco , onani mafunso atatu otsatila . Mafunso angatithandize kudziŵa zimene munthu amakhulupilila . 2 : 1 - 12 . N’kofunika kuonetsa makhalidwe onse amenewa paumoyo wathu . ” ( Mat . 16 : 19 ) Mwacitsanzo , mu 36 C.E . , Petulo anali na mwayi wolalikila uthenga wabwino kwa Koneliyo ndi a m’banja lake . Limanena kuti Yesu anapeleka “ mapemphelo opembedzela . . . kwa amene anali wokhoza kumupulumutsa ” ndipo “ anamumvela . ” Ndi umboni wotani umene Paulo anapeleka ponena za kuuka kwa Yesu ? ( Sal . 10 : 14 ) Niyamikila kwambili onse amene anayesetsa kunithandiza mwa kunilembela mfundo pamisonkhano , kuphunzila cinenelo camanja , ndi kunimasulila nkhani m’cineneloci . Timakondwela kugwilitsidwa nchito ndi Yehova mosasamala kanthu kumene tikutumikila . ( Afilipi 4 : 5 ) Kukhala woganiza bwino kungatithandize kuika maganizo athu pa kulambila Yehova m’malo moganizila kwambili za thanzi lathu . Mkristu sangafunikile kufunafuna cuma m’dzikoli limene lipita posacedwapa cabe kuti ‘ asamalile banja lake . ’ ( 1 Yoh . Patapita mwezi umodzi , ndinamuyankha kuti ndifuna kumudziŵa bwino coyamba . Conco , n’nangoyang’ana pansi ndi kucoka pamene tinali kuti nikaganizilepo pa zimene ananiuza . NYIMBO : 73 , 119 Kodi tingaonetse bwanji kuti ndife nzika zokhulupilika za Ufumu wa Yehova ndi kukhala m’banja lake la ana angwilo ? 7 : 1 - 5 ) Limeneli ndi phunzilo lofunika kwa ife . N’cifukwa ciani anthu ambili sadziŵa tanthauzo la zimene zikucitika m’dzikoli ? Nkhani yotsatila idzafotokoza mmene mungacitile zimenezi . 26 : 52 ) Pakati pa mahandiledi a abale athu amene ali m’ndende pali Isaac , Negede , ndi Paulos amene akhala m’ndende ya ku Eritrea kwa zaka zoposa 20 . Adzathandiza anthu omvela kumasuka ku ukapolo wa ucimo ndi imfa kuti akhale angwilo . — Ŵelengani Chivumbulutso 22 : 1 , 2 , 17 . Koma Yehova anacenjezanso kuti , kwa kanthawi , colengedwa cauzimu cimene cinakamba na Hava kupitila mwa njoka , cidzalimbana ndi anthu okonda Mulungu . — Gen . Hamilton ) , Na . Ni aukali ndipo amakayikila munthu aliyense . Kodi Yehova anapatsa anthu mwai wotani pambuyo pa Cigumula ? Tinali kuyembekezela a Komiti Yoona za Nchito Yolemba Mabuku amene anali atatsala pang’ono kuloŵa . Mouzilidwa , mtumwi Yohane analemba kuti : “ Mulungu ndiye cikondi . ” Ndipo pamene tilalikila , timakhala ngati tikuwauza kuti : ‘ Takubweletselani mphatso yabwino kwambili . Popita mu ulaliki , muziwatengako abale ndi alongo amenewa . Conco , kuti apitilize kuwafika pamtima anafunika kusintha - sintha ulaliki wake malinga ndi zosoŵa za anthu . N’cifukwa ciani tasintha kamvedwe kathu ? ( b ) Fotokozani citsanzo coonetsa kuti Yehova amacita zinthu mokoma mtima kwambili pothandiza anthu opanda ungwilo . Ni mayeselo ati amene Rudolf Graichen anakumana nawo ? Kukamba zoona , ulamulilo wa Yehova ni wofunika kuucilikiza na mtima wathu wonse . Kodi colinga cathu ciyenela kukhala ciani pamene tiphunzitsa munthu Baibo ? “ Anathyola cipatso ca mtengowo n’kudya . 7 : 1 - 3 ) Kenako , Aramagedo isanacitike , Yesu adzawapatsa mphoto yao ya kumwamba . Conco , modzicepetsa Yesu anasambitsa mapazi awo . Nthawi zina ukalamba umacititsa munthu kuvutika maganizo . Kumasulila Cituvalu kunali kovuta cifukwa panalibe mabuku ena amene tingafufuzemo mau ena kuti atithandize . Tonsefe timacita cidwi tikaganizila mmene maselo a thupi la munthu amagwilila nchito modabwitsa . Conco , mwana wanga wina na mkazi wake ananitenga kuti nizikhala nawo . Pamene anakhazikitsa ansembe mu Isiraeli , Aroni ndi ana ake anapakidwa magazi a nkhosa yaimuna munsi mwa khutu la kulamanja , pa cala cacikulu ca kumanja , ndi ca kumwendo wa kulamanja . Kodi nimakhala wotangwanika ngako na zocita za tsiku na tsiku cakuti nimakhala na nthawi yocepa yopemphela kapena kuŵelenga Baibo ? ’ Yelekezelani kuti Yehova akuuza inu mawu amenewa . Baibo inalonjeza kuti : “ Yehova sadzataya anthu ake . ” 25 : 1 - 30 ) Potsilizila , anakambanso za ena amene adzacilikiza abale a Khiristu ndi kukhala ndi moyo pa dziko lapansi kwamuyaya . M’bale amene akutumikila monga woyang’anila dela ku South Africa anati : “ Kucokela pamene ana athu aakazi anabadwa , ndinali kupemphela nao usiku uliwonse kupatulapo ndikapita kwina . ( Miy . 1 : 5 ) Conco , tifunika kudalila malangizo anzelu a m’Baibo ndi kupempha Yehova kuti atitsogolele . Kuona zolakwa moyenelela kudzatithandiza kuthana nazo bwino ngati zacitika . Wakuti iye anadzipeleka kwa Yehova cifukwa cokhala na cikhulupililo mwa Khristu , amene anaukitsidwa . Iwowa anagulidwa kucokela mwa anthu , monga zipatso zoyambilila zopelekedwa kwa Mulungu ndi kwa Mwanawankhosa . ” Kucita zimenezi kudzakuthandizani kusunga malumbilo anu acikwati , ndipo mudzakhala acimwemwe . Baibulo limati “ Mulungu ndi cikondi . ” Conco , mofulumila n’nayankha kuti “ Nifuna ! ” Ndipo anthu ambili amakhulupilila kuti Mboni za Yehova zilidi ndi coonadi , cifukwa zimasiyana ndi zipembedzo zimene zimalekelela makhalidwe oipa . Kodi Baibo ili na uphungu wanji pa mfundo ya kulamulila mkwiyo ? [ 1 ] ( ndime 14 ) Onaninso nkhani yakuti “ Despite Trials , My Hope Has Remained Bright ” mu Galamukani ! ya Cizungu ya April 22 , 2002 , imene ifotokoza mbili ya Andrej Hanák wa ku Slovakia . Kodi mau a Paulo angawalimbikitse bwanji anthu amene amadziona ngati osafunika ? Caka ciliconse timasindikiza ndi kutumiza mabaibulo ndi mabuku ofotokoza Baibulo mamiliyoni ambilimbili . Mmodzi wa iwo anali Simon Atoumanos , wansembe amene anakhalako mu ulamulilo wa Byzantine m’zaka za m’ma 1360 . Patapita caka cimodzi cabe , tinapemphedwa kuti tikatumikile ku Northern Ireland . Panthawi imeneyo , anthu ambili a Mulungu anali kuyembekezela kuyenda kumwamba ndi kukakhala mafumu ndi ansembe pamodzi ndi Yesu . 20 : 5 ) Ngakhale anthu amene amaganiza kuti amalambila Mulungu m’njila yoyenela ndi akapolo a zikhulupililo zonama ndi miyambo yacabecabe . ( Sal . 73 : 28 ) Mzimu wa Yehova udzayamba kugwila nchito pa wophunzila Baibulo wacidwi ameneyo . Hezekiya Cifukwa cakuti m’mawa tsiku limenelo kunagwa cimvula cacikulu , madzi a mtsinjewo anasefukila . Ngakhale n’conco , okwatilana afunika kupewa makhalidwe oipa amene ali paliponse m’dzikoli . Mungaonenso Danieli 2 : 44 ; ndi Mateyu 6 : 9 , 10 . Kodi munadzifunsapo kuti umoyo wanu na banja lanu udzakhala bwanji kutsogolo ? Ambili amakonza zakuti tsiku lina pa kulambila kwawo kwa pabanja , azitambako JW Broadcasting . N’kuthekanso kuti iye anamvela zakuti Yesu anaukitsa mwana wa Yairo . ( Aef . Koma anthu ambili sanali kukambanso za maloboti . Akatelo , m’pamene munthuyo amakhala woyenelela kubatizika . ( Agal . 3 : 16 ) Koma cifukwa cakuti Yehova salephela kukwanilitsa malonjezo ake , anthu amenewa adzaukitsidwa na kukhala ndi moyo wangwilo m’paradaiso padziko lapansi . — Sal . ( Aroma 7 : 21 - 23 ) Malinga ndi mbili , anthu acita zinthu zoipa kwambili zimene zabweletsa mavuto aakulu kwambili . Tikamalalikila uthenga wabwino kwa anthu ena , timawathandiza kuti asakaonongeke pamene dziko la Satanali likuonongedwa . Mwacionekele , Baibulo nalonso likupezeka m’cinenelo cimene mumamvetsetsa , mosasamala kanthu za kumene mumakhala kapena mtundu wanu . Kodi anali kupita naye kuti ? Timakumana ndi mavuto ambili paumoyo masiku ano . Mufunse mmodzi wa Mboni za Yehova . Yehova sakanakhala ndi mlandu akanapanda kutumiza Mwana wake pa dziko lapansi kuti adzapeleke dipo . Yesu anafotokoza kuti “ mbeu yabwino ” imaimila “ ana a Ufumu . ” Ndipo “ namsongole ” amaimila “ ana a woipayo . ” Moyo ndi mphatso yamtengo wapatali . Koma io anapitilizabe kulalikila ndi kubatiza ophunzila . Mlongo wina ku France anati : “ Nkhani zakuti ‘ Kodi Zinangocitika Zokha ? ’ Tinaimilila pafupi ndi cibafa cacikulu comwelamo ziweto , cimene munalinso madzi ozizila . Koma limaonetsanso kuti samakhalila kungodziŵa zinthu zokhudza alambili ake . ( Salimo 139 : 6 ; Aroma 11 : 33 ) Mulungu amawadziŵa bwino kwambili anthu kusiyana ndi kompyuta imene imangosunga zinthu zokhudza anthuwo . Makolo angaonetsenso kulimba mtima mwa kuthandiza ana awo kudziikila zolinga zauzimu ndi kuzikwanilitsa . Kucita zimenezi kumalimbitsa ubwenzi wanu ndi iye . — Aheb . Ngakhale kuti ciŵelengelo ca anthu amene anapenyelela seŵeloli sicidziŵika bwinobwino , lipoti la kumapeto kwa cakaco linaonetsa kuti anthu oposa 1 miliyoni analipenyelela . Munthu Amene Mumakonda Akamwalila , Na . Koma kaŵili - kaŵili kumaphatikizapo kum’phunzitsa makhalidwe abwino , amene angam’thandize kupanga zosankha zabwino kuyambila ali mwana . Mwacitsanzo , atumwi anakwapulidwa cifukwa colalikila za Khristu . Yehova anamuyankha mosapita m’mbali kuti : “ Popeza ndidzakhala ndi iwe , udzaphadi Amidiyani ngati kuti ukupha munthu mmodzi . ” ( Ower . 6 : 11 - 16 ) . Mwacionekele , anaphunzila zambili kwa makolo ake na azimbuye ake . ( Yak . 3 : 17 , 18 ) Timapeza cimwemwe ngati tiyesetsa kupanga ubwenzi ndi anthu ocokela m’maiko ena , kuonetsa mzimu wololela kwa anthu a cikhalidwe cina , kapena kuphunzila citundu cawo . M’malomwake , Yosefe ndi Mariya anamupeza akukambilana mau a Mulungu ndi aphunzitsi pa kacisi . — Luka 2 : 45 - 47 . Timayamikila kwambili mwai wathu wogwila nchito ndi Mulungu m’masiku ano otsiliza . Posadziŵa zimene tingakambe kwa anthu ali m’mavuto , tingacite manyazi ndi kuyamba kuwapewa . Cifukwa cakuti mumacita zimenezo mwa kufuna kwanu osati cifukwa cakuti munthu wina wakukakamizani . ( b ) Fotokozani mmene kunyada kungasokonezele mtendele mumpingo . Muziwalangiza mwacikondi . Cimeneci cinali cocitika capadela cifukwa Koneliyo sanali m’Yuda komanso anali wosadulidwa . Mu nkhani za mtsogolomu , tidzaona mmene cikhulupililo ca Yosefe cinamucititsila kukhala wofunika kwa Mulungu wake Yehova ndi kwa banja lake lovutalo . Koma sikuti cimeneci cinali cozizwitsa cothela cimene Mulungu anacita kupitila mwa Elisa . Ganizilani cimene cinacititsa kuti Paulo alembe mau a pa 2 Timoteyo 2 : 19 . Ngakhale kuti Aisiraeli anaputa mkwiyo wa Yehova , Mose ndiye anakwiya . Koma chimo limenelo munthu akhoza kucotsedwa nalo mumpingo ngati nkhaniyo siinathetsedwe . N’cifukwa ciani tifunika kupewa misece ? Masomphenya Oonetsa Amene Ali Kumwamba 4 5 : 22 - 24 ; Afil . 4 : 5 ) Angafunikenso kuganizila ngati mwamuna wakeyo nthawi zonse amamuletsa kupita muulaliki , kapena ndi tsiku limenelo cabe limene wam’pempha kuti asapite . ( Onani cithunzi cili kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Nanga ndi mafunso ati amene tikambilane ? Koma panopa , aliyense wa ife ali ndi Baibulo lake lake . 1 : 1 - 3 ; Yes . Ine n’nauzidwa kuti nizisonkhana mumpingo wa ku Bronx . Pambuyo pake ndinacita manyazi kwambili . ” Mkazi wanga Gloria anali kutsuka mkati , ine n’nali kutsuka kunja . “ Udalitsike Cifukwa ca Kulingalila Bwino Kwako ” ( Abigayeli ) , June 119 : 133 . Ocita kafukufuku ena amanena kuti acinyamata a masiku ano ndi “ M’badwo Wodzikonda . ” Ndinabadwila ku Hungary , mumzinda wa Székesfehérvár , umene wakhalapo kwa zaka zoposa 1,000 . Amadziŵa kuti kukhala owoloŵa manja ndiyo njila yopezela cuma “ ceniceni . ” Kuukila mwacindunji kuli monga cimphepo camphamvu cimene cacitika mwadzidzidzi ndi kuononga nyumba yanu nthawi imeneyo . Zimenezi zandithandiza kudziŵa kuti ndili ndi luso lapadela limene ndingagwilitsile nchito potumikila Yehova . ” Pang’ono ndi pang’ono analoŵetsa ziphunzitso zabodzazo mumpingo m’malo mwa coonadi ca m’Mau a Mulungu . Kodi n’ciani cinamuthandiza kuti ayambe kukhala mwamtendele ndi ena ? Nanga ni mfundo ziti za coonadi zimene imwe mumakonda ngako ? Conco , kuika zinthu zauzimu patsogolo ni njila yoonetsela kuti mumamuyamikila Mulungu cifukwa ca madalitso amenewa . Iye angacotse munthuyo mumpingo ngati waona kuti afunika kucita zimenezo . Ndinayankha kuti , “ Mwafunsa funso losavuta , ndipo ndikuuzani . ” Koma Ahabu sanali kuganizila za Malamulo a Yehova ngakhale pang’ono . Tisanakhale Akhiristu , tinali kucita macimo , ndipo mwina sitinali kudziŵa mmene Mulungu anali kukhumudwila na zocita zathu zoipa . Iye ndi munthu woipa wauzimu . Ngati timakondadi abale athu , tidzapewa kuwasungila zifukwa akatilakwila . ( Ŵelengani Miyambo 30 : 4 . ) ( Mateyu 13 : 36 - 43 ) Pa nthawi yaitali imeneyo , panali Akristu oona ocepa . Iwo anaumitsa mitima yawo na maganizo awo , ndipo ufulu umene anakhala nawo atatulutsiwa mu Iguputo , anali kungouseŵenzetsa pokhutilitsa zofuna zawo na zilakolako zawo . — Aheb . Atangozindikila kukwanilitsidwa kwa ulosi wa m’Baibo , io analengeza molimba mtima kwa anthu ena kuti Ufumu wa Mulungu wayamba kulamulila . 12 Mungakhale na Moyo Kwamuyaya Padziko Lapansi Cinamuvuta kukhulupilila zimene zinam’citikila . M’bale Pranas , amene tamuchula poyamba , anati : “ Ungakambe zinthu zambili kwa ana ako , koma io amangoona zimene umakonda kucita ndipo amatengela zimenezo . ” Kodi Akristu Ayenela Kupita ku Tuakacisi Topatulika Kukalambila ? Cikumba ca nyama n’colimba kupambana gumbwa , koma cimawonongeka ngati sicinasamalidwe bwino , kapena ngati caikidwa pamalo otentha kwambili , a cinyontho , kapena padzuŵa . ( Yobu 14 : 14 , 15 ) Anthuwo akadzaukitsidwa , adzakhala osangalala ndi athanzi . 14 Mbili Yanga — N’natsimikiza Mtima Kukhala Msilikali wa Khristu Yehova sanalenge anthu ndi ufulu wakuti azidzilamulila okha popanda citsogozo cake Kodi n’ciani cikanathandiza Akhristuwo kupilila m’nthawi zovuta zimenezo ? — 1 Pet . Ambuya nawonso ananilimbikitsa kupita , ndipo n’napitadi . SARA anaŵelamuka na kuyang’ana capatali . ( Luka 11 : 13 ; Agalatiya 5 : 22 , 23 ) Tikamacita zimenezi , Yehova adzatithandiza kudziŵa zimene zimam’kondweletsa ndipo tidzayamba kuona zinthu mmene iye amazionela . Tiphunzilapo kuti Yehova angathe kutithandiza m’njila imene sitinali kuyembekezela . Ndiyeno , mmodzi wa ana athu aakazi anatiuza kuti panthawi yopumula ku sukulu , acinyamata ena a Mboni amacita zosangulutsa zina zimene iye amaona kuti ndi zosayenela . Conco woyang’anila ndende anatipatula kwa akaidi ena . Sicisunga zifukwa . Iye pofuna kudziŵa zimene zinali mumtima mwa abale ake , sanadziulule kwa iwo pamene anabwela ku Iguputo kudzagula cakudya . ( Miy . 2 : 13 ) Anatipatsa nzelu zopanga mapulani , na kudziŵa mowakwanilitsila mapulaniwo . Sitingasithanitse mwayi umenewu na cina ciliconse . Cifunilo canu cicitike , monga kumwamba , cimodzimodzinso pansi pano . ” — Mateyu 6 : 9 , 10 . Kodi nimaona kuti kufatsa ni mantha ? Mmodzi wa alendowo anali mkulu waciyela . Malemba amakamba mosapita m’mbali kuti Yehova amaona okalamba okhulupilika kukhala amtengo wapatali , ndipo amafuna kuti atumiki ake aziwalemekeza . ( Sal . 22 : 24 - 26 ; Miy . * Ufumuwo utakhazikitsidwa , Satana ndi ziŵanda zake anathamangitsidwa kumwamba na kuponyedwa padziko lapansi . Izi zingaticititse kufunsa kuti : ‘ N’ciani cinamucitikila pambuyo pake ? ’ ( Dan . 2 : 4 ) Izi zionetsa kuti mzimu woyela ungathe kutikumbutsa mfundo zimene tinaŵelenga ndi kuzisunga bwino mosungilamo cuma cathu . — Luka 12 : 11 , 12 ; 21 : 13 - 15 . Kodi munthu wakuthupi na munthu wauzimu amasiyana m’njila zina ziti ? Ndi cocitika capadela citi cimene cinacitika mu 2013 ? N’nali mu ukapolo . ” kutsogolelewa ndi Mau a Mulungu ? Anacita zinthu zoonetsa kuti coonadi cimene anaphunzila cinam’fika pa mtima . M’malo mwake , io anangocita zimene anaona kuti n’zabwino . ( 1 Timoteyo 4 : 15 , 16 ) Analimbikitsanso Timoteyo kuti sayenela kulola unyamata wake , mwinanso manyazi kumulepheletsa kukhala wolimba mtima pocita zinthu zoyenela . 1 : 19 , 20 . Iye amagwila nchito mwakhama , ndipo anthu amamukonda cifukwa cakuti amagwila nchito mwaluso . Nafenso tiyenela kuyesetsa kudyetsa mtima wathu cakudya cauzimu cogwilizana ndi zosoŵa zathu . M’malo mwake , Yesu anali kuwacenjeza za zimene zingadzawacitikile ngati angalephele kukhala okonzeka ndi kukhala maso . Yesu anadziŵa kuti mavuto amene anali kukumana nao anali akanthawi , koma madalitso amene adzalandila kumwamba adzakhala amuyaya . ( Yoh . 3 : 22 ; 4 : 1 , 2 ) Mofanana ndi ubatizo wa Yohane , nawonso ubatizo wocitidwa na ophunzila a Yesu unali cizindikilo cakuti munthu walapa macimo amene anacita posamvela Cilamulo ca Mose . Tikakhala omvela masiku ano , cidzakhala cosavuta kutsatila malangizo pa “ cisautso cacikulu , ” pamene dongosolo lonse loipa la Satana lidzaonongedwa . Banja limeneli linapita m’zambili . Zinali kudzatheka cifukwa cakuti anali kudzaukitsidwa . Ndipo iye anandipatsa zosowa zanga zonse . Ndipo malipoti anaonetsa kuti mbali zonse za utumiki wakumunda zinawonjezeka . Kodi malangizo amene Paulo anapeleka ku mpingo wa ku Roma angatithandize bwanji pakabuka mikangano ? Kodi muli ndi cocitika cofanana ndi cimeneci cimene cinalimbitsa cikhulupililo canu ? ( b ) Ndi mafunso ati amene tiyenela kudzifunsa ? KUFATSA Yehova anauza Aisiraeli kuti : “ Mau anga adzatsika ngati mame , ngati mvula yoŵaza pa udzu . ” Popeza kuti Demetiriyo anali mmodzi wa nthumwi za Yohane , kapena woyang’anila woyendela , ayenela kuti anamveketsa bwino zimene Yohane analembela Gayo . ( Yos . 23 : 14 ) Mwa kupenda mbili ya kukhulupilika kwake , anthu amene amam’konda ndi kumumvela angakhale ndi cidalilo cakuti iye adzasunga lonjezo lake lozikidwa pa mfundo ziŵili ngakhale akumane ndi mayeselo : ( 1 ) Iye sadzalola mayeselo aliwonse kufika pamene sitingakwanitse kuwapilila , ndipo ( 2 ) ‘ adzapeleka njila yotipulumutsila . ’ ( Akol . 3 : 2 ) Ndithudi , abale a Kristu anafunikila kuika m’maganizo coloŵa cao cosaonongeka cimene ‘ anawasungila kumwamba . ’ — Akol . Cinsinsi Namba 9 Umunthu Wanu Ayenela kupempha Yehova kuti awatsogolele ndi kuwapatsa mphamvu kuti apilile mavuto amene akumana nawo . Sitikudziŵa cimene cinayambitsa mkanganowo , koma Paulo mokhumudwa anawauza kuti : ‘ Kristu wakhala wogawanika ’ pakati panu . M’njila ina , Baibo ili ngati toci ya mphamvu imeneyi . ( 2 Pet . 3 : 9 ) Nthawi zambili , tikamva mau amenewa timaganizila za anthu amene akuphunzila coonadi . Ŵelengani Yesaya 40 : 26 . Ndiponso , tiyenela kukonda Mulungu ndi ‘ maganizo athu onse , ’ kutanthauza nzelu zathu zonse . Kodi wopambana onse pa kupeleka mphatso n’ndani ? Kodi Manowa anacita ciani atamva kuti adzakhala kholo ? ( Yohane 17 : 3 ) Nkhani ino , iyankha mafunso otsatilawa : Kodi kaŵelengedwe kathu kayenela kukhala kotani kuti tizisinkhasinkha bwino ? Ganizilaninso maboma amene amalimbikitsa nkhondo ndi ciwawa pakati pa mitundu yosiyana - siyana ya anthu . Maboma ena amapondeleza anthu wamba osauka , ndiponso amakonda ziphuphu ndi tsankho . Komabe , pali anthu ambili amene amaona kuti ciphunzitso cimeneci si coona . Nkhawa Zokhudza Banja 6 “ Ngakhale kuti simunamuonepo , mumamukonda . ( Sal . 92 : 7 ) Conco , n’zosadabwitsa kuti masiku ano , anthu ambili satsatila mfundo za makhalidwe abwino . Ulemu waconco , umaoneka wacikale masiku ano . Komanso , taganizilani zimene zingacitike tikakumana ndi mavuto . Iye anayambanso kupemphela nthawi zonse . Baibo siimachula cabe mfundo zimenezo . Koma pali zina zimene tiyenela kucita . Mumadana ndi onse ocita zopweteka ena . ” Mwacitsanzo , anthu anali kukhala mwamantha cifukwa coopa atsogoleli acipembedzo amene anali kuwanamiza ndi kupanga malamulo ambili olemetsa . ( Mat . 23 : 4 ; Maliko 7 : 1 - 5 ; Yoh . 2 : 11 - 14 ) Nanga imwe mungawapeputsileko bwanji akulu udindo wawo wopeleka uphungu ? Iye anaonetsa kuti anali wodzikuza mwa ‘ kusabwezela zabwino zimene anacitilidwa . ’ N’nali kumuona kuti n’citsanzo cabwino pankhani yogonjela otsogolela m’gulu . Ŵelengani Levitiko 8 : 5 , 6 . Nanga n’cifukwa ciani ndimamvela malamulo a Mulungu m’malo motengela makhalidwe oipa a m’dzikoli ? Cikondi cimeneci “ sicitha , ” kutanthauza kuti cimapitiliza kukhalapo nthawi zonse , ndipo m’kupita kwa nthawi cimakula . Iye anazindikila kuti , “ Onsewo anali kukonda kupemphela kwa Mulungu . ” [ Cithunzi papeji 29 ] Modzicepetsa Eliya anasankha Elisa kukhala womulowa m’malo ( b ) Kodi imwe mwapindula bwanji na mfundo za m’Malemba zimene timaphunzila pa misonkhano yathu ? Mpake kuti Baibo imati , “ wodala ndi mtundu umene Mulungu wawo ndi Yehova , anthu amene iye wawasankha kukhala colowa cake . ” — Sal . ( Deuteronomo 30 : 19 ) Kodi Hezekiya anagwilitsila nchito bwanji ufulu umenewo ? Kodi Mulungu adzalola kuti anthu apitilize kupondelezana ndi kucitilana nkhanza ? Iyai . M’fanizo lake lonena za tiligu ndi namsongole , Yesu anakambilatu za mdima wa kuuzimu umene unali kudzacititsidwa ndi ampatuko . Nanga Yehova anacitanji ? Kuti mumve zambili zokhudza gulu la Mulungu padziko lapansi , onani buku lakuti Jehovah’s Witnesses — Proclaimers of God’s Kingdom . [ Cithunzi papeji 20 ] Munaphunzilanso mmene mungapitilizile kucita zinthu zimene zimakondweletsa Mulungu pamene muyembekezela moyo wosatha . — Yak . Mtumwi Paulo anauza Atesalonika kuti : “ Ifeyo timakunyadilani ku mipingo ya Mulungu cifukwa ca kupilila kwanu ndi cikhulupililo canu pokumana ndi mazunzo ndi masautso onse amene mukulimbana nao . ” ( 2 Ates . Nikumbukila kuti tsiku lina n’naŵelenga mau m’buku linalake amene sanali kucoka m’maganizo mwanga . Kuti aweluze mogwilizana na cilungamo ca Mulungu , anafunika kudziŵa ngati munthuyo anapha mnzake “ atamubisalila ” ndiponso “ cifukwa codana naye . ” 4 : 8 ) Sizokhazo , Atate wathu wakumwamba watipatsa mwayi wokhala m’gulu lake . Akanena zimenezo , tingamuuze kuti : “ Limenelo ndi fanizo labwino . Pa Ekisodo 21 : 22 pali nkhani ya amuna aŵili amene akumenyana . Ndiyeno wina avulaza kwambili mkazi wapakati cakuti mkaziyo wabeleka mwana nthawi isanafike . Akristu oona anali kudzaonetsa bwanji kuti ndi “ anthu odziŵika ndi dzina [ la Yehova ] ” ? Baibulo limati : “ Mutu wa mwamuna aliyense ndi Kristu . Mutu wa mkazi ndi mwamuna . ” ( 1 Akor . Pakufunika anchito a zomangamanga , odziŵa kujambula mapulani a nyumba , a luso pa zopangapanga , oyang’anila nchito yomanga , oyeza malo , okonza mapaipi a madzi , odziŵa kuochelela zinthu , okonza za magetsi , odziŵa kugwilitsila nchito zimagalimoto zokumbila , akalipentala , odziŵa kubzala ndi kusamalila maluŵa , ndi odziŵa kukongoletsa malo . Tifunika kukumbukila kuti tonse tili na zofooka , ndi kuti pali zinthu zina zimene timacita bwino . Kodi n’zimenenso imwe mufuna ? Kodi mukufuna kudziŵa zimene Mboni za Yehova zimakhulupilila ? Yesetsani kuona zimene mungaphunzilepo pa zimene mwalakwitsa . Ngati mwayamba kucita izi mukali wamng’ono , sipatenga nthawi itali kuti muone kuti Yehova akukutsogolelani , kukutetezani , na kukudalitsani . Kodi Yehova sadzalola Mkristu kusoŵa cakudya ? Ufunika kugwilitsila nchito njila iliyonse . Ndinauza amai kuti : “ Musadandaule , io adzalema kukuletsani . ” Yesu anati : “ Aliyense woyang’anitsitsa mkazi mpaka kumulakalaka , wacita naye kale cigololo mumtima mwake . Mwacitsanzo ndinaphunzila zimene Baibulo limanena pa 1 Akorinto 6 : 10 kuti : “ Akuba , aumbombo , zidakwa , olalata , kapena olanda , onsewo sadzaloŵa mu Ufumu wa Mulungu . ” “ Ciliconse cili ndi nthawi yake . ” — MLAL . Pamene n’nali wacicepele , n’nali kukonda kuŵelenga nkhani zopeka za sayansi . Ngati simunadzipatulile na kubatizika , mungacite bwino kuganizila kufunika kocita zimenezi . Patangopita nthawi yocepa , ndinapatsidwa mwai wocezela mipingo monga woyang’anila dela . Wamalonda mu fanizo ili amaimila anthu oona mtima amene amacita khama kuti apeze zosoŵa zao za kuuzimu . Ngati mai ndi mwana wake sanafe , mwamuna wa mkazi wovulazidwayo sanali kuloledwa kubwezela . Kodi mwatsimikiza mtima kufunafuna cuma cauzimu ? Nthawi ina Davide ali kwawo , atate ake , a Jesse , anamutuma kuti akaone azikulu ake , amene anali m’gulu la asilikali a Sauli . ( Yeremiya 31 : 20 ) Mulungu amamvela cimodzi - modzi ndi alambili ake masiku ano . Nimatonthozedwa na lonjezo la Mulungu lakuti adzabweletsa Paradaiso mmene zinthu zonse zidzakhala “ zatsopano ” kuphatikizapo manja anga . Patapita nthawi , zimene Mariya anakamba kwa wacibale wake Elizabeti zionetsa kuti anali munthu wauzimu kwambili . Tsopano tiyeni tione mmene tingakambitsilane ndi mwininyumba zimene Malemba amanena . Palibe cimene tingacite kuti matenda ao athe . N’cifukwa ciani mikangano imeneyi inalembedwa m’Baibulo ? NKHANI YA PACIKUTO | KODI MUNGAKONDE KUPHUNZILA BAIBULO ? 12 : 2 ) Kodi Yehova anam’dalitsa bwanji ? Ndi maganizo otani amene Habakuku akanakhala nao ? N’cifukwa ciani kukanakhala kupanda nzelu kuganiza conco ? Ophunzila anabwela kwa Yesu kuti amuuze za vuto la cakudya . Koma Yehova sasintha , ndipo amaonabe kuti cilungamo na cifundo n’zofunika kwambili . Amuna anga akhala akunithandiza kulimbana ndi vuto imeneyi . ” Yehova Mulungu akuthandiza anthu ambili kumasuka ku ukapolo wokoka fodya kupyolela m’nchito yophunzitsa anthu ya padziko lonse . N’nali kumvetselako zimene anali kukambilana , ndipo nthawi zina n’nali kupita ku misonkhano ya mpingo pamodzi na amayi . Tiyeni tikambilane maulosi ocepa cabe amene ni zizindikilo za “ masiku otsiliza . ” ( b ) N’ciani cingatithandize kupambana polimbana ndi zofooka zathupi ? Abulahamu anadziŵa kuti Yehova sangasinthe mwadzidzidzi ndi kukhala wankhanza . Koma m’kupita kwa nthawi , iye anakhulupilila kuti Yesu anali Mesiya cifukwa ca umboni wokhutilitsa umene anapeza . Iwo atasonkhana pa Phili la Sinai , Yehova anacita zizindikilo zazikulu zoonetsa kukhalapo kwake . Apa mfundo ya Yesu inali yakuti cinthu cofunika kwa iye pa nthawiyo , cinali kuthandiza Ayuda monga mmene anali atauzila ophunzila ake . ( Salimo 83 : 18 ) Sitikanalandila mphatso kucokela ku gwelo la ulamulilo . 1 Samueli caputa 16 - 30 ; 2 Samueli caputa 1 - 24 ; 1 Mafumu caputa 1 - 2 ( Yoh . 17 : 17 ) Caciŵili , “ ndife anchito anzake a Mulungu , ” ndipo watipatsa mzimu woyela kuti utitsogolele . ( 1 Akor . 3 : 9 ; Mac . 34 : 13 , 14 ) Monga kholo , kodi cimeneci ndiye colinga canu ca kuuzimu ? NYIMBO : 51 , 58 Malamulo amenewo anaphatikizapo lamulo lokhudza kulalikila . Iwo amatsogolela mu ulaliki ndi kuthandiza mipingo m’njila zina . Atumiki a pa Beteli amatumikila pa ofesi ya nthambi kapena m’maofesi omasulila mabuku . Anthu ambili ku Japan amakonda kalembedwe kameneka cifukwa n’kosavuta kuŵelenga . Kwa nthawi yoyamba , mawailesi a m’dziko la Mexico anagwilitsidwa nchito kufalitsa uthenga wabwino m’dziko lonselo . Pambuyo pamsonkhanowo , woyang’anila nthambi watsopano anayamba kutsogolela nchito yolalikila . Ndinali kukonda kunama mabodza ndi kucita zinthu zacinyengo za mtundu uliwonse . Ambili amadela nkhawa kuti akadzafika pa zaka zopumula panchito sadzakwanitsa kupeza ndalama zokwanila zogulila zinthu zimene amafuna . Kodi n’kutheka kuti uthenga womveka bwino ndiponso wofunika kwambili womwe uli m’fanizoli unali kuphimbika ndi zinthu zing’onozing’ono zimenezo ? Ambili a io takhala tikusonkhana nao , ndipo ena amakonda kuphunzila nafe Baibulo , koma safuna kutumikila Mulungu . Iye amalandila munthu wocokela mu mtundu uliwonse , amene amamuopa ndi kucita cilungamo . ” Samueli anali ataona kale ana 7 a Jese , koma Yehova anamuuza momveka bwino kuti sanasankhepo aliyense wa iwo . Kodi mphamvu za Satana n’zazikulu bwanji ? Yohane sanaone munthu wakufa pa mtanda . Ndinamuuza kuti ndifuna Baibulo la cikatolika cabe . 6 : 8 , 9 . Mabuku athu ofotokoza Baibulo amafalitsidwanso m’cinenelo cimeneci . Ndipo n’zimenedi n’nacita . CIKWATI ni mbali ya umoyo . Komabe , anthu amakalamba m’njila zosiyanasiyana . Yehova amaona atumiki ake onse okhulupilika kuti ndi amtengo wapatali , kuphatikizapo acinyamata . — Salimo 148 : 12 - 14 . Eduardo anati : “ Ndidziŵa kuti nthawi imene ndinali kutali ndi banja langa sindingaibweze , koma sindimaganizila kwambili zinthu zakumbuyo . 17 : 31 ) Mulungu anasankha Yesu kukhala Woweluza wathu , ndipo tili ndi cidalilo cakuti adzaweluza mwacilungamo ndi mwacikondi . — Ŵelengani Yesaya 11 : 2 - 4 . Ganizilani mmene mkazi wamasiye anamvelela pamene analoŵa m’kacisi ndi tumakobidi tuŵili twatung’ono . M’nthawi za m’Baibulo , cikwati ca pacilamu , kapena kuloŵa cokolo , unali mwambo wakuti mwamuna akwatile mkazi wa m’bale wake wopanda ana , kuti abeleke ana ndi colinga cakuti dzina la banja la m’bale wake lisafafanizike . — Gen . Mungasonyezane cikondi , koma mwa njila yoyenela . Zilizonse zimene banja lacikristu lingasankhe posamalila makolo okalamba , onse ayenela kutsimikizila kuti zosankha zao zilemekeza dzina la Mulungu . ( Yes . 61 : 1 , 2 ; Luka 4 : 17 - 21 ) Conco , iye anali munthu wacifundo cacikulu , anali kumvetsetsa mavuto amene anthu anali kukumana nawo , ndipo anali wofunitsitsa kuwathandiza . — Aheb . Izi n’zimene katswili wina wa pa Univesiti ya Nebraska ku United States analemba pambuyo popenda zotsatila za kafukufuku wina wa za umoyo . Zimene Yakobo anacita zinali ndi tanthauzo labwino kwambili ndipo Yosefe anakhudzidwa kwambili ndi cikondi cimene bambo ake anamuonetsa . Hans ndi Brook atamva zocitika zolimbikitsa zimene anzawo amene anatumikilako ku maiko ena anawasimbila , anaganiza zoyenda ku dziko lina kukacita upainiya . ( Genesis 17 : 17 ) Iye anadabwa na kukondwela kwambili . Tiyeni tikambilane zimene zili pa Mateyu 14 : 14 - 21 . Nkhani imeneyi ipezekanso mu Nsanja ya Olonda ya February 1 , 2012 , masamba 18 - 21 . Tingatengele citsanzo ca Yehova mwa kupewa kuda nkhawa kwambili ngati zinthu sizinayende mmene tinali kuyembekezela . ( Luka 19 : 12 ) Yesu sanalandile mphamvu zonse monga mfumu atangofika kumwamba . Imeneyo idzakhala nthawi ‘ yoima cilili ndi kuona Yehova akutipulumutsa . ’ N’cifukwa ciani anthu ena afunika kuona kuti tinadzipatulila kwa Yehova ? Mwacionekele , pali zifukwa zimene mumawaonela conco atumwi amenewa . N’lothandiza pa mbali ziti ? Amaganiza kuti munthu afunika kukhala wopanda mantha ndi waukali . N’ciani cinamuthandiza ? ( Ŵelengani Salimo 62 : 8 ; 1 Petulo 5 : 7 . ) A Daka : Ndinaona kuti mumakhulupilila zimenezi . Koma ku Burkina Faso ndinali mlendo , ndipo anthu ambili anali kudabwa akandiona . Mtumwi Paulo anati : “ Cikondi cimene Kristu ali naco cimatikakamiza . ” N’naphunzila kuti pali njila zambili zocitila zinthu . “ Kumbukila Mlengi wako Wamkulu . ” — MLAL . Ndipo muzionanso kuti Mulungu wakulonjezani zimenezi inuyo pa nokha . Ndipotu cakudya cimene ndidzapeleke kuti dzikoli lipeze moyo , ndico mnofu wangawu . ” — Yohane 6 : 48 - 51 . Mulungu tinalibe naye nchito . 6 : 34 ; Sal . Umu ndi mmene amandikumbutsila kuti ndifunika kulemba mayankho akuti iye akayankhe pa misonkhano ya mpingo wa Cikristu pa mbali ya mafunso ndi mayankho . Komanso ‘ anamvetsetsa ciliconse ’ cimene Mulungu anali kufuna kuti iwo acite . ( Miy . Baibulo limati : “ Mukhale otsanzila anthu amene , mwa cikhulupililo ndi kuleza mtima , akulandila zinthu zimene Mulungu analonjeza monga colowa cao . ” Imfawe , mphamvu yako ili kuti ? ” — 1 Akorinto 15 : 55 . Conco , Mulungu anaonetsa Zekariya masomphenya otsilizila pofuna kutsimikizila Ayuda kuti amawakonda ndiponso kuti adzawateteza akayambanso kugwila nchito yake . Anafunanso kuwayamikila pa zonse zimene anacita . Pa zocitika ngati zimenezi , zolengedwa zakumwamba ndiye zinali kuyamba kulankhula ndi anthu . Inu Yehova , conde tipulumutseni . . . . Petersburg ku Russia umene unali ndi mtumiki wothandiza mmodzi ndipo unalibe mkulu . M’malomwake , tiziganizila mau a pa Salimo 136 : 23 amene aonetsa kuti Yehova amatikonda nthawi zonse . Lembali limati : “ Iye amene anatikumbukila pamene adani anatinyazitsa . ( Yuda 3 ) Kuti tidziŵe mmene tingacitile zimenezi , tiyeni tiphunzile mmene Yefita ndi mwana wake anapililila mavuto pa umoyo wao . Cifukwa cakuti timaphunzila Mau a Mulungu , timadziŵa kuti maulosi ambili akukwanilitsidwa masiku ano . ( 1 Akor . 10 : 13 ) Tizikumbukila mau apa Afilipi 1 : 29 akuti : “ Munapatsidwa mwai . Osati mwai wokhulupilila Kristu wokha , komanso wovutika cifukwa ca iye . ” Nimaleka kugwila nchito yofunikila kuti ningokhala cabe , kapena kuti nitambe TV . “ M’masiku otsiliza kudzakhala onyodola , . . . amene azidzati : “ Kukhalapo kwake kolonjezedwa kuja kuli kuti ? Pambuyo pa zaka ziŵili , mmodzi wa aja amene anavomela kuloŵa usilikali , anali pa gulu la asilikali amene anasankhidwa kukapha Mboni zokhulupilika . Atamwa mkakawo , Sisera anagona tulo tofa nato . Mkulu wina anali kukonda kucezela abale a m’gawo lake mwacidule akapita mu ulaliki , kuti adziŵe za umoyo wawo . Zimenezi sizicitika pamlingo waukulu conco mu mpingo wacikhiristu . Ngakhale n’conco , mavuto a m’banja akuwonjezeleka pakati pa anthu a Mulungu . Kodi a “ khamu lalikulu ” akucita ciani masiku ano ? Nanga ndi madalitso otani amene io adzalandila posacedwapa ? ( Gen . 19 : 16 ) Citsanzo cimeneci cionetsa kuti Yehova amadziŵa bwino mavuto amene anthu ake okhulupilika amakumana nawo . — Yes . Kodi Yehova adzacitapo ciani pa mavuto amene tikumana nawo ? Atapita kumeneko , anateteza uthenga wabwino . ( Mac . Kodi amakaikila ngati malamulo a Mulungu ndi othandiza ? Kodi kudziŵa mphamvu za Satana kuli na ubwino wanji ? Kumatithandiza kukhala na kaonedwe koyenela ka maboma a anthu . 63 : 7 - 9 ; Yak . Panthawi imodzi - modzi , amalemekeza na mtima wonse maudindo amene Yehova wapeleka kwa ena . Gavin anakamba kuti sanali kudziŵa zambili zokhudza Baibulo , ndipo sanafune kuti ena adziŵe zimenezo . Ngakhale n’conco , kungakhale kulakwa kutenga cisomo ca Mulungu kukhala cifukwa cocitila zoipa . Mwacitsanzo , tingakhale na maganizo monga akuti : ‘ Ngakhale nicimwile Mulungu , siniyenela kuda nkhawa kweni - kweni . ( Eks . 10 : 28 ) Mose asanacoke pamaso pa Farao analosela kuti mwana wamwamuna woyamba wa mfumu adzafa . 3 : 18 - 21 ) Mosakayikila , na imwe mungavomeleze kuti kuseŵenzetsa malangizo ouzilidwa a Paulo amenewa kungapindulitse mwamuna , mkazi , ndi ana . 3 : 23 , 24 . Pambuyo pake dokotala angakupatseni cithandizo ca mankhwala coyenela . TSAMBA 3 • NYIMBO : 14 , 109 M’fanizo limeneli , Yesu anakamba kuti anamwali anayenela kukhala okonzeka , ndipo nyali zao zinafunika kukhala zoyaka mpaka mkwati atafika . Kaya takhala Mboni kwa utali wotani , tiyenela kupitilizabe kusintha umunthu wathu . — 2 Akorinto 13 : 11 . ( 2 Mbiri 29 : 1 - 11 , 18 - 24 ; 31 : 1 ) Patapita nthawi , pamene mfumu ya Asuri , Senakeribu inafuna kuononga Yerusalemu , Hezekiya anacita zinthu molimba mtima ndiponso mwa cikhulupililo . N’zomvetsa cisoni kuti mavuto amene anthu akulu - akulu amakumana nawo , nthawi zambili amavuta kuthetsa . 3 : 1 - 4 ) Kodi nchito yoyendela ndi yoyeletsa imeneyo inatenga utali wotani ? Mwacionekele , iye anali kukonda kusinkhasinkha ndi kukamba mau oyamikila pa zinthu zabwino zimene Mulungu anam’citila . Anthu amenewa sanapatsidwe matalente amene Yesu anapatsa akapolo ake odzozedwa . ( Habakuku 2 : 3 ) Ganizilaninso citsanzo ici : Yehova anapeleka dipo , ndi kulonjeza kuti adzatikhululukila macimo athu . Olemba nkhani ambili akale anali kukometsela nkhani kuti akondweletse mafumu awo na kukweza mtundu wawo . Conco , kwa zaka 10 n’nakulila kutali na amayi ndi ambuya . ( Akolose 4 : 6 ) Khalani woganizila ena ndi wolimbikitsa . Mulungu atalenga anthu , anafuna kuti io akhale padziko lapansi kwamuyaya ndi kuti asamadwale kapena kufa . ( Sal . 145 : 18 ) Kukhulupilila Yehova mwa njila imeneyi kudzatithandiza kupilila mavuto oyesa cikhulupililo amene tingakumane nawo . Mu 536 B.C.E . , anthu a Mulungu anatsiliza kumanga maziko a kacisi . Gulu limeneli lidzapulumuka pamene dziko la Satana lidzaonongedwa . ( 2 Tim . ( Maliko 10 : 17 , 18 ; Yoh . 7 : 16 ) Yesu sanali kulankhula ndi ophunzila ake m’njila yowapangitsa kuzimva kuti ndi acabecabe kapena otsika kwambili . TENGELANI CIKHULUPILILO CAO | RABEKA Anthu amene amaŵelenga Baibulo amam’dziŵa Pontiyo Pilato cifukwa ca zimene anacita pamene Yesu anali kuimbidwa mlandu mpaka kuphedwa . ( Mat . Mosakaikila Baibulo limagwilitsila nchito maina osiyana ponena za kuukila kumodzi . Conco , khalani olimba m’cikhulupililo ndipo mulimbane naye Satana . Nili na mkazi wanga mu 2011 ( Oweruza 11 : 34 - 37 ) Atatewo anaona kuti mwana wao anali ndi cikhulupililo ndipo anasangalala kwambili cifukwa anadziŵa kuti kudzipeleka kwa mwana wao kudzakondweletsa Yehova . ( Aef . 5 : 1 ; 1 Pet . 2 : 25 ) Makamaka makolo ayenela kudziŵa maonekedwe a nkhosa zao , amene ndi ana ao okondedwa . Ndipo ayenela kuyesetsa kuwatsogolela kuti akalandile madalitso a Yehova a mtsogolo . Popeza kuti panali “ pakati pa usiku , ” zinali zovuta kupeza anthu ogulitsa mafutawo cifukwa munali m’mbuyo mwa alendo . Munthuyo akuweluzidwa kuti ni wolakwa cifukwa ca umboni wonama wopelekedwa ndi anthu odziŵika kuti ni opanda pake . Acibululu na mabwenzi ake akhumudwa ndipo asoŵa mtengo wogwila . Buku la Yobu limaonetsa kuti kuona zinthu moyenela n’kofunika ngako . Buku limeneli ni limodzi mwa mabuku a m’Baibo oyambilila kulembedwa . ( b ) Ndi pa cocitika citi pamene mungamve monga mmene Mose anamvelela ? Popeza zimenezi n’zimene angakwanitse kucita , Yehova amakondwela nazo . Iye amadziŵa kuti abale ndi alongo athu amam’konda , ndi kuti amafunitsitsa kukhala Mboni zake . ( 2 Timoteyo 1 : 4 ) Mofanana ndi Paulo , zioneka kuti Timoteyo anaphunzila ‘ kulila ndi anthu amene akulila , ’ n’colinga cakuti awatonthoze ndi kuwalimbikitsa . Pokhala otsatila a Kristu ndiponso Mboni za Yehova , timazunzidwa padziko lonse . Nikaona mmene amayi alemekezela atate , zimanilimbikitsa kutengela khalidwe lawo . ” Mwina tingadzakambilane funso limeneli nthawi ina . Anthu amenewa amakonda kukamba za Mulungu . Koma bwanji ngati mumvela monga mmene m’bale wina dzina lake Aaron anali kumvelela ? Fotokozani mmene Mulungu anaseŵenzetsela Elisa pa ciukililo cacitatu cochulidwa m’Baibo . Filip ndi Ida , amene ali pa banja ndipo anacokela ku Denmark , nthawi zambili anali kulakalaka kusamukila kudela lina kumene kufunika ofalitsa ambili . 8 , 9 . ( a ) Ni mapulojekiti aphindu ati amene mungakonde kucitako ? Ngakhale ndi conco , sindinapeze mayankho a mafunso amene ndinali nao okhudza Mulungu . Njila ina imene mungaonetsele kuwala kwanu ni mwa kulimbikitsa mgwilizano m’banja lanu na mumpingo . Kodi kusinkhasinkha kumatanthauza ciani ? Iwo akutumikila monga oyang’anila a madela ndipo akuthandiza abale ndi alongo ambili m’mipingo . ( Mat . 9 : 22 ) Akatswili a Baibo amakamba kuti mau a Ciheberi ndi a Cigiriki amene anawamasulila kuti “ mwanawe , ” amatanthauzanso “ kukoma mtima na cifundo . ” Ciwonongeko ca Yerusalemu sicinali codabwitsa kwa anthu okhala mmenemo . N’naona kuti Yehova wayankha pemphelo langa . Kodi pemphelo limalimbitsa bwanji ubwenzi wathu ndi Mulungu ? N’ciani cinacititsa Marita kukhulupilila kuti mlongosi wake Lazaro adzauka ? Mwa ici , akulu - akulu a boma ananipeleka ku khoti kaŵili konse , koma mlandu unatuluka washauti . Erin , amene amakhala ku South Africa anakamba kuti : “ Pamene tinali ana tinali kukonda kudandaula cifukwa cophunzila Baibulo , kusonkhana , ndi kupita mu utumiki . Mwacibabwa , anthufe timafuna kukhala ndi thanzi labwino , ndipo timafunanso kuti anthu amene timakonda akhale ndi thanzi labwino . ( Deuteronomo 17 : 18 ) Kuonjezela apo , okopela malemba aluso analemba mipukutu yambili cakuti pofika m’nthawi ya atumwi , Malemba anali kupezeka m’masunagoge a m’dziko lonse la Isiraeli , ngakhale kutali kwambili ku Makedoniya . Kuphunzitsa wina coonadi n’kosangalatsa kwambili ( Onani ndime 7 ) Nanga bwanji masiku ano ? M’nkhani yoyamba tidzakambilana za ciyambi ca cikwati , mmene Cilamulo ca Mose cinatsogolela cikwati , ndi mfundo imene Yesu anakhazikitsa yokhuza cikwati . ( Ŵelengani Aheberi 6 : ​ 4 - 9 ; yelekezelani ndi Deuteronomo 30 : 19 ) Cenjezo lake linali lacindunji , koma iye analinso ndi cidalilo cakuti io adzalandila mphoto yao . Mulungu anafuna kuti ana awo akhalenso ndi ana anzawo mpaka dziko lonse kudzala ndi anthu . ( a ) N’cifukwa ciani tiyenela kukhala oleza mtima ndi okoma mtima ? Kodi zinthu zina zimene tingacite kuti tipite patsogolo mwauzimu n’ziti ? M’pomveka kuti Mulungu anakonza zakuti awononge anthu aciwelewele amenewo . ( 2 Pet . Kodi anthu ambili akamba zotani pambuyo polandila Baibulo lokonzedwanso la 2013 ? Koma m’kupita kwa nthawi , cifukwa ca kufooka kwa thanzi la Lene , tinaganiza zokukila ku dziko lotentha . Mwacitsanzo , ganizilani zimene zinacitika pamene mnzake wapamtima Lazaro anamwalila . Udzanena kuti : “ Ndipita kukaukila dziko lokhala ndi midzi yopanda mipanda . pa jw.org , pa kamutu kakuti , ZOKHUDZA IFEYO > MAFUNSO OFUNSIDWA KAŴILIKAŴILI . Ofesi ya nthambi inatipempha kusamukila ku mpingo watsopano ku Irlam . Mu 1935 , panali kusintha kwakukulu kumene kunakhudza mmene Cikumbutso cinayenela kucitidwila mtsogolo , popeza tanthauzo la “ khamu lalikulu ” lochulidwa pa Chivumbulutso 7 : 9 , linafotokozedwa momvekela bwino . Koma Arthur anaona kuti afunika kucoka ndithu . Ngakhale pamene ana anu aoneka monga safuna kukamba , imeneyo ndiye nthawi imene amafuna kwambili kukambilana ! N’cifukwa ciani kulimbitsa cikhulupililo n’kofunika kwambili ? Bwanji ponena za zinthu zakumwamba monga nyenyezi ndi mapulaneti ? Solomo atamwalila , mwana wake Rehobowamu anakhala mfumu . Zinthu zinafika poipa kwambili cakuti n’nali kucita kulaka - laka kuti mkazi wanga acoke panyumba kuti nitambe bwino mavidiyo a zamalisece . ” Macmillan , tsamba 69 ) Nchito imeneyi ikucitikadi masiku ano . Paulo anauzilidwa kulemba kuti Abulahamu anali kukhulupilila kuti Mulungu ali na mphamvu zoukitsa Isaki kwa akufa . 4 : 1 , 7 ) Conco , sitiyenela kusunga mkwiyo , umene uli ngati poizoni , m’ziwiya zosungilamo zinthu zamtengo wapatali . 28 : 1 - 6 ) Yesu anali wamoyo . Iye sanali kudziŵa zimene Baibulo limakamba . Conco , anaganiza zoyamba kuliŵelenga . Koma m’zaka zambili zokatifikitsa ku 1914 , odzozedwa anali kumasuka mu ukapolowo . — w16.11 , mapeji 23 - 25 . Mkatewo , umene Yesu anayelekezela ndi mana amene Aisiraeli anakana , ungatibweletsele madalitso osatha . Conco , nikayamba kulalikila , nimapemphela ca mumtima kwa Yehova . Nimam’pempha kuti anithandize kuona munthuyo mmene iye amamuonela . Mwacitsanzo , mwana wa sukulu wa zaka 15 anaombela ana a sukulu anzake a m’kalasi mwao , ndipo anapha anthu aŵili n’kuvulaza anthu 13 . Inu mukanakhala Mkristu panthawiyo , tsiku lililonse mukanakhala ndi mantha akuti mwina mungamangidwe ndi kumenyedwa . Kodi mukupindula ndi zitsanzo za anthu okhulupilika a mumpingo mwanu ? Ine ndi mng’ono wanga tinatsimikizila makolo athu kuti tidzaŵasamalila akadzakalamba . Cifukwa amatikonda , timamva kukhala osungika kulikonse kumene tingam’tumikile m’gulu lake . ( Oweruza 5 : 6 , 7 ) Anthu anali kubisala m’nkhalango ndi m’maphiri . N’cifukwa ciani tifunika kukhala olimba mtima ? Kodi adzasangalala mpaka liti ? 19 : 6 , 7 . Mtunduwo unali kudzatulutsa Mesiya , amene adzaphwanya Satana ndi kutsimikizila kuti Yehova ndiye woyenela kulamulila . ( Gen . ( Miy . 8 : 13 ) Kaya tili pa utumiki wanji pali pano , tidziŵe kuti kuyenda ndi Yehova ndiwo mwayi woposa wina uliwonse . Nsanja ya Olonda yacingelezi ya September 15 , 1950 , inafotokoza kuti nthawi zina munthu , cocitika , kapena cinthu cinacake m’Baibulo cinali kuimila cinthu cina cacikulu mtsogolo . Mtumwi Yohane analemba kuti tifunika kusonyezana cikondi “ ceni - ceni m’zocita zathu . ” Kuti mudziŵe zambili , pemphani a Mboni za Yehova a m’dela lanu kapena pitani pa webusaiti yathu ya www.jw.org . Popeza kuti tonse sitinali kudziŵa kuyendetsa , tinapempha amene anatigulitsa kuti atibweletsele motokayo . Zopinga zitaculuka , Aisiraeli anagwa ulesi na kuleka nchitoyo , ndipo anayamba kugwila nchito zawo za panyumba ndi za kuminda . Ngakhale kuti Baibulo limatilimbikitsa kugwila nchito modzipeleka , limanenanso kuti tifunika “ kutsimikizila kuti zinthu zofunika kwambili ndi ziti . ” Komabe Yakobo anapitiliza kuganizilapo pa mau a Yosefe . “ M’badwo umapita ndipo m’badwo wina umabwela , koma dziko lapansi lidzakhalapobe mpaka kalekale . ” — Anatero MFUMU SOLOMO WA M’ZAKA ZA M’MA 1000 B.C.E . Ndipo cofunika kwambili n’cakuti anali kutumikila Yehova ndi zolinga zabwino . Ni njila yabwino kwambili yoonetsela kuti timakonda Yehova na kumuyamikila . Njila imodzi imene Mulungu amatitonthozela ni kupitila mwa “ mzimu woyela . ” Kodi N’zoona Kuti Davide Anamenyana Ndi Goliyati ? ‘ Kodi cikumbumtima canga cimandicenjeza ndikamayesedwa ? ’ Akhristu amafuna - funa Ufumu wa Mulungu na cilungamo cake . Panthawi inayake , zinthu zinasintha kwambili mu umoyo wa Yobu . ( a ) Kodi mtumwi Paulo analemba mfundo iti yokhudza kusamalila makolo ? Amacita izi poseŵenzetsa makina a m’ndeke olongoza malo . Conco , kugwila nchito maola amenewo kunandithandiza kucita upainiya wa nthawi zonse . Anthu ambili amakamba kuti popeza kuti Yesu sanali Mlevi , iye sakanaloledwa kuimilila pamwamba pa nyumba yopatulika ya pakacisi . Ena anatsala opanda ciliconse . Akhristu ali na makhalidwe abwino . — Ŵelengani Malaki 3 : 18 . Aliyense wa iwo amamvetsela maganizo a mnzake mwaulemu , ndipo capamodzi amapeza njila yothetsela vutolo , imene onse angakhutile nayo . ” 2 : 13 , 14 ) Yehova ndiye anauzila Paulo kulemba nkhani zonsezi , ndipo ndife otsimikiza mtima kuti n’zolondola . Abusa a machalichi acikristu salalikila za Ufumu wa Mulungu . Kodi munakhumudwapo cifukwa ca kucotsedwa nchito ? Zinali zolimbikitsa kwambili kuonana ndi abale ndi alongo 20 amene anatumikilako monga amishonali m’dziko la Portugal . 1 : 28 ) Yehova sanalenge anthu mamiliyoni panthawi imodzi . Adamu ndi Hava anafunika kubeleka ana ndipo naonso ana ao anafunika kubeleka ana mpaka kudzaza dziko lapansi . Munthuyo anathandizidwa ndi Msamariya , munthu amene anali kulemekeza Cilamulo ca Mose , koma amene sanali kuyanjidwa ndi Ayuda . — Yohane 4 : 9 . Abale ambili anali osauka koma tinali kusangalala kuŵayendela . Iye anali wolimba mtima . Abale ambili anali kucokela kumidzi yakutali , kumene masitima sanali kufikako , ngakhale miseu kunalibe . 8 : 44 ) Satana ndi mdani wathu wamphamvu kwambili . Tiyeni ticite khama kumabwelelako kwa anthu acidwi , ndipo ngati n’kotheka , tiziphunzila nao Baibulo ndi kuwathandiza kuti akadzipeleke ndi kubatizika . Kuyambila caka ca 2000 ine ndi Anita tikukhala m’mzinda wa Elkilstuna m’dziko la Sweden , kumene takhala tikuthandiza anthu olankhula Ciluya kuphunzila Baibulo . Pewani Kutengela Maganizo a Dziko , Nov . ASAYANSI amagwilitsila nchito zipangizo ndi ndalama zambili kuti adziŵe zamtsogolo . Mwacitsanzo , amafuna kudziŵa mmene kuonongedwa kwa mpweya kudzakhudzila dziko lapansi . Amafunanso kudziŵa ngati mvula idzagwa kudela lanu tsiku lotsatila . Conco , mu January 1960 , tinayamba utumiki wathu wa zaka zambili pa Beteli . Akhiristu a m’zaka 100 zoyambilila , anaphunzila kucotsa udani umene unakhazikika pakati pawo . Imodzi mwa mamapu amenewo kaonekedwe kake n’kacilendo , ndipo ali pa mpukutu wa m’zaka za m’ma 1200 wochedwa Beatus wa ku Liébana . Komabe , makhoti aciyuda sanapatsidwe mphamvu zakuti azipha zigaŵenga . Aroma okha ndiwo anali na mphamvu yocita zimenezo . Kodi Yesu anati ciani ponena za “ cisautso cacikulu ? ” Nanga cidzayamba bwanji ? Mfundo zake siziloŵedwa m’malo na cidziŵitso catsopano . Iye ndi mkazi wake anagaŵilanso magazini a Galamukani ! Mfundo za m’Baibulo zingatithandize kuphunzitsa bwino cikumbumtima cathu pankhani ya zosangulutsa . NYIMBO : 69 , 70 Nkhani ziŵilizi zifotokoza mmene munthu amadziŵila kuti wasankhidwa kuti akakhale kumwamba ndiponso cimene cimacitika munthuyo akadzozedwa . ‘ Cangu na Cikondi Zinawonjezeka Kwambili ’ ( msonkhano wacigawo mu 1922 ) , May MUKAGANIZILA za Marita mlongo wa Lazaro , kodi muona kuti iye anali munthu wotani ? Kapena amangomangika ndi kuti anzake safuna kuceza naye ? Panthawi imeneyo , panali patapita zaka zambili Nowa ndi Yobu atafa kale , koma Yehova anali kukumbukilabe kukhulupilika kwao . Banja lingakambitsilane kaya makolo angapitilize kukhala okha malinga ngati pali thandizo lina . Mtima wao wakhala wacinyengo . 10 : 34 ) Pambuyo pake , Petulo analemba kuti Mulungu “ amafuna kuti anthu onse alape . ” Komabe , masiku otsiliza ano , nchito ingapangitse anthu kukhala na nkhawa kwambili . Koma , kodi timadziŵa bwanji kuti nthawi zokwanila 7 zimenezi zinathadi mu 1914 ? ( a ) N’ciani cimene Yehova wacita cimene cimatikokela kwa iye ? Ni zitsanzo za Mboni za Yehova ziti zimene zikupilila mosangalala cizunzo ? Mwina mukufuna kucita upainiya . Anthu onsewa anali na mwayi ‘ wolapa na kutembenuka . ’ ( Mac . Popeza kuti ndinali kuwakonda ndi kuwakhulupilila , ndinamvela malangizo ao . M’kalata yake yopita kwa Timoteyo , mtumwi Paulo analemba kuti “ masiku otsiliza ” adzakhala “ nthawi yapadela komanso yovuta . ” 5 : 13 ; 20 : 6 ) Yesu adzaphwanya mutu wa njoka ndi kuthetselatu mavuto onse obwela cifukwa ca kupanduka kwa Satana . — Gen . Thanzi yanga siili bwino olo pang’ono . ” Mwacitsanzo , mnyamata wina wa ku Brazil anavutika kwa zaka zambili kuti athetse cilakolako coipa . Patangopita mawiki ocepa , Arthur analandila foni yocoka ku ofesi ya nthambi ya Britain , yom’pempha kuti adzayambe kugwila nchito ya m’dela tsiku lotsatila . Kukhala wocenjela kumasiyana ndi kukhulupilila zonse zimene tamvela . MPINGO wacikristu wa m’nthawi ya atumwi ku Kolose unali pa mavuto . Makhalidwe abwinowo , amene ndiwo cipatso ca mzimu , amatipatsa cithunzi ca mmene alili Mulungu wamphamvuzonse . Ndipo nthawi zambili Nani anali kugwa pa njinga yake pobwela kudzandiphunzitsa . Tingadzifunse mafunso monga awa : ‘ Kodi nimaona zosangalatsa kukhala zofunika ngako kuposa misonkhano na ulaliki ? Ngati anthu ayamba kutsutsana pankhani inayake , monga yakuti amuna ndi akazi okhaokha azikwatilana kapena ya kucotsa mimba , auzeni zimene Mau a Mulungu amanena ndiponso zimene inu mumacita potsatila malangizo amenewo . Mnyamatayo anauza msilikali kuti iye anali ndi cilolezo cokhalila m’dzikolo , koma akawalala anamubela ziphaso zoyendela na ndalama . ABALE AMENE AKALAMILA : Ndi Mboni za Yehova zokha zimene zikukwanilitsa ulosi wa Yesu wakuti uthenga wabwino udzalalikidwa padziko lonse . Ndiyeno , cilengezo citapelekedwa ku mpingo , onse anakondwela kwambili . ▪ Cifukwa Cake Tifunika Kukhala Oyela Yesetsani kusaganizila kwambili mmene zakukhudzilani . Kapena kodi ningacite ciani ngati anthu ena osawadziŵa anipempha kuti nicite nawo masewela a pa intaneti ? ’ Ngakhale kuti Baibo yacitilidwa nkhanza zonsezi , siinasinthe . Ni umboni wanji umene umatipatsa cidalilo cakuti n’zotheka kufulatila macimo ? Pamene ndinapitiliza kuphunzila Baibulo , ndinazindikila kuti tonse ndife osoŵa mwa kuuzimu , ndi kuti tiyenela kukhala odzicepetsa kuti tipeze zosoŵa zathu . Coyamba , kumbukilani kuti Nowa anayenda na Mulungu kwa zaka zambili m’dziko loipa Cigumula cisanafike . Panthawiyo , nayenso Tony anali kuphunzila Baibo na Mboni za Yehova . Izi zinacititsa kuti liziŵelengedwa ndi anthu ocepa . ( Salimo 41 : 4 ) Davide anadziŵa kuti Yehova anamukhululukila macimo ake ndipo anadalila Yehova pamene anali kudwala . Mwacibadwa , timafuna kutsimikizila umboni wa zinthu ndi kudziŵa ngati zinthuzo zidzacitikadi . Cifukwa codzikuza , Uziya anapita kukacisi kukagwila nchito ya ansembe imene siinali nchito yake . Ansembe 81 anafika ndi kumuletsa . 12 : 26 . Tangoganizani , anthu amene anatamba seŵelo imeneyi m’caka ca 1914 cokha , anali ambili kupambana alaliki a Ufumu onse amene alipo lelo . ( 1 Sam . 1 : 24 - 28 ) Kumeneko “ Mwanayo Samueli anapitiliza kukula , akukondedwa ndi Yehova . ” ( 1 Sam . Kaŵilikaŵili , anthu opsinjika maganizo amafuna kungowaonetsa cifundo m’malo mowauza zocita . Yobu anali kudziŵa bwino mfundo za Mulungu . Kodi umoyo wawo wakhala bwanji ? Conco , iye anawauza za “ Mulungu amene anapanga dzikoli ndi zinthu zonse zili mmenemu . ” Kodi si zoona kuti ndi mwai kuonetsa anzathu cikondi m’njila yapadela imeneyi monga alengezi a Ufumu ? MMENE MALEMBA AMACIFOTOKOZELA CIKONDI Komabe io anangomulambalala osam’thandiza . ( Ŵelengani Akolose 3 : 5 , 6 . ) Kuyelekezela mmene timaonela nchito yathu yakuthupi ndi mmene timaonela zinthu zauzimu kungatithandize kudziŵa zimene timakonda kwambili . M’malo moyang’ana zakumbuyo , Sara anayang’ana za kutsogolo . Iye sangakupatseni cinthu ciliconse cabwino mukam’tsatila cifukwa alibe cabwino . Poyamba , anthu a m’banja lakewo anakhumudwa , kenako anam’kwiila kwambili . Mariya ‘ anadabwa kwambili ’ na mau amenewa . Iye sanadziŵe kuti n’cifukwa ciani mngeloyo anali kukamba naye . ( Mateyu 24 : 45 - 47 ) Mofanana ndi m’nthawi ya atumwi , Yehova ndi Yesu masiku ano akudyetsa kapena kuti kuphunzitsa anthu ambili pogwilitsila nchito anthu ocepa . Iwo anadziŵa kuti angacite zambili mu utumiki wa Yehova , koma anali kunyalanyaza kucita zimenezo . Kodi thandizolo linagwila nchito ? ( b ) Kodi mapemphelo amene mlongo wina anapeleka analimbitsa bwanji ubwenzi wake ndi Yehova ? Kodi tingakhale bwanji “ ngati akufa ku ucimo ” ? Kodi cikhulupililo n’ciani ? N’zoona kuti si nthawi zonse pamene kucitila umboni kumakhala kopepuka . Kwa zaka 33 , ine ndi Angie tinali mu utumiki woyang’anila dela ndi zigawo . Ndipo mumzinda wina kumeneko anakumana ndi mwamuna wina amene anali ndi matenda oopsa a khate . Komabe , palibe ‘ cida cimene cingapangidwe ’ cimene cidzalepheletsa nchito yolalikila za Ufumu ndi kupanga ophunzila . Hava anaonetsa mtima wodzikonda pofuna kukhala ngati Mulungu . ( 1 Yoh . 5 : 14 ) Komabe , njila yaikulu imene Mulungu amatikokela kwa iye ndi kupyolela mu dipo . Mwa kukamba zabodza zokhudza Yehova , Satana ananyozela dzina lopatulika la Mulungu . — Gen . Kufatsa kumakondweletsa Yehova . Acicepele ambili acikhristu akukumana ndi ciyeso ngati cimene Yosefe anakumana naco . N’cifukwa ciani cikhulupililo n’cofunika kwambili ? Kodi lemba la Mateyu 7 : 12 lingatithandize bwanji kuzindikila malo oyenela kukambitsilana ndi anthu , nthawi yokambilana nao ndi mmene tingakambilane nao ? Ndipo kucokela pamene anthu anacimwa , Yehova wakhala akutsimikizila atumiki ake okhulupilika kuti adzalandila madalitso amene Adamu anataya . Iye akukhazikitsa mtendele m’dziko lako . ” ( 2 Samueli 11 : 2 - 4 , 14 , 15 ; 1 Mbiri 2 : 16 ) Yowabu anali m’bale wa Abisai , conco n’kutheka kuti Abisai anamva zimene Davide anacita . Komabe , cofunika kwambili si mmene anali kuonekela kweni - kweni , koma mmene timudziŵila masiku ano . N’cinyengo cabe . KODI COLINGA CA MGWILIZANOWU N’CIANI ? Bungwe lina lalikulu la mgwilizano wa zipembedzo limadzitama kuti lili ndi mamembala a zipembedzo zoposa 200 zocokela m’maiko 76 . Tonsefe akulu ndi ana , amuna ndi akazi , a pabanja ndi amene sali pabanja , tingacite bwino kutsanzila cikhulupililo cake . Poyambitsa mwambo wa Cikumbutso , Yesu anauza atumwi ake kuti amwe vinyo amene anali kuimila magazi ake . ( Mat . Mukalibe kuyankha , mungacite bwino kudziŵa mmene Baibo imayankhila mafunso atatu awa : Kodi mmene munthu anapangiwila zimaonetsa ciani ponena za kutalika kwa nthawi imene munthu afunikila kukhala na moyo ? N’cifukwa ciani cikhulupililo n’cofunika ? Mwina maganizo anu amathamangila ku cibalo kapena mkwapulo . Maganizo otelo amasangalatsa Satana cifukwa iye amafuna kuti tisamakondane ndi kugwilizana . Kodi lemba la Salimo 118 : 22 linakambilatu za cocitika capadela citi ? Nkhani zothandiza Akristu amene akudwala ndi amene akusamalila odwala zinafalitsidwa mu Galamukani ! Nayenso Stéphanie wocokela ku France anati : “ Nchito yapadelayi inatiphunzitsa kuti cimene cimatigwilizanitsa si cikhalidwe kapena citundu , koma ndi kukonda kwathu Yehova . ” Kapena akanaopa cifukwa cakuti anali wamng’ono ndi wosakhwima ? Alongowo anatiphunzitsa coonadi ca mtengo wapatali cokamba za Yehova na colinga cake kwa anthu . Koma Yesu sanacite zimenezo . Kuona Zolakwa Moyenelela , Na . Tinali kumwa madzi oipa ndipo nthawi zambili tinali kudya mphodza ndi maegipulanti . Anapanganso dzuŵa , mwezi , ndi nyenyezi . ” Ni ufulu wanji umene Yehova anapatsa anthu ake Aisiraeli ? Sheryl ndi mng’ono wake John ( Onani ndime 13 ) Poyankha , Yesu anakamba fanizo limene linaonetsa kuti panalibe kusiyana pakati pa anthu osakhala Ayuda ndi “ tiagalu . ” Zoonadi , Yesu ali ndi mphamvu kwambili . ( Mac . 5 : 33 - 39 ) Mlandu wathu unafalitsidwa m’nyuzipepa , ndipo abale ndi alongo 49 anaikidwa m’ndende . ( Mlal . 9 : 11 ) Munthu angapezeke m’ngozi cabe cifukwa cakuti zangocitika mwa tsoka . Koma Sara anali kulambila Mulungu woona , Yehova . M’madela ena , timalephela kulalikila m’manyumba ena a mafulati kapena a kumipanda . Ndi malangizo amene Yesu anapeleka pamene anati : “ Zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inunso muwacitile zomwezo . ” ( Mat . Ngakhale kuti Yehova kupitila mwa Yehu anapatsa uphungu Yehosafati , sanalephele kuona “ zinthu zabwino ” mwa mfumuyo ( Onani ndime 8 ndi 9 ) William , amene tamuchula m’nkhani yapita , anati : “ Munthu amene ndinali kumuseŵenzela kale amagwila nchito pamlingo woyenela . 55 : 4 ) Nayenso Danieli anauzilidwa kulemba za kubwela kwa “ Mesiya Mtsogoleli . ” ( 2 Akor . 12 : 7 ) Ngati apitiliza kucilimika kuti akhale ndi khalidwe labwino , angakhale ndi cidalilo cakuti adzapambana . Ngakhale n’telo , tingaphunzile zambili kwa Rabeka . Ndipo Mkhiristuyo angakhale ndi mafuno abwino kwa mnzake wocokayo , akuti m’tsogolo akabweze mtima kuti akapitilize cikwati cawo , ndi kuti akakhale Mboni . Ndi pangano lotani limene Yesu anapanga ndi ophunzila ake okhulupilika ? Anthu a m’zipembedzo pafupi - fupi zonse zikulu - zikulu — Akhristu , Ahindu , Ayuda , Asilamu , ndi ena — amakhulupilila kuti munthu ali na mzimu umene sukufa . Amakamba kuti munthu akafa , mzimuwo umacoka ndi kukakhala na moyo kumalo a mizimu . Yesu anakambilatu kuti : “ Anthu adzakupelekani kumakhoti aang’ono , ndipo adzakukwapulani m’masunagoge ndi kukuimikani pamaso pa abwanamkubwa ndi mafumu . ” Ulosi wolembedwa pa Chivumbulutso 12 : 7 - 12 umafotokoza kugwilizana kwa zocitika zoipa zimene zakhala zikuononga mtundu wa anthu ndi kubadwa kwa Ufumu wa Mulungu . Goliyati anayamba kufuula mwaukali . Paulo analangiza Akhiristu kutengela cikhulupililo ca amene anali kutsogolela pakati pawo . 14 , 15 . ( b ) N’cifukwa ciani mufunika kuyesetsa kuti mukapezeke m’dziko latsopano ? ( Machitidwe 17 : 28 ) Kuzindikila mfundo imeneyi kumatithandiza kupewa kuika moyo wathu paciswe , kaya tikuseŵenza , kuyendetsa motoka , kapena kucita zosangalatsa . Yehova anathandiza Ophunzila Baibulo kumvetsetsa coonadi cofunika ca m’Malemba cimene cinali citabisika cifukwa ca ziphunzitso zabodza za cikristu ca dziko . ( Mac . 2 : 8 . ) Ngakhale amishonale amene atumikila m’dziko lina , amadziŵa kuti sangadalile cabe mfundo zing’ono - zing’ono zimene amamvelako pamisonkhano . Yehova amaseŵenzetsa abale kuti aziphunzitsa mumpingo . Conco , abale onse ayenela kunola luso lawo lokamba nkhani . N’cifukwa ciani tiyenela kupemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele ? Kukhala wansangala kungakuthandizeni kucepetsa nkhawa . Mulungu anam’funsa kuti : “ Anapatsa munthu pakamwa ndani , kapena ndani amapanga munthu wosalankhula , wogontha , woona kapena wakhungu ? 10 : 4 ) Komabe , anthu ena samakhulupilila Mulungu cifukwa ca mavuto aakulu amene io kapena anthu ena amakumana nao . Pamene Mulungu anaononga dziko la kale la ciwawa m’nthawi ya Nowa mwa kubweletsa Cigumula , ndi anthu ocepa cabe amene anapulumuka . Panthawi imeneyi , n’nali na mwayi wotumikila ndi mlongo Etta Huth , amene anali mayi wanzelu . Iwo anaona kuti Mulungu anawasamalila mwacikondi mwa kuwapatsa cilimbikitso cauzimu pa nthawi yake . NYIMBO : 90 , 87 NYIMBO : 95 , 13 ( Ŵelengani Luka 10 : 21 . ) Kuwonjezela pamenepo , waphunzitsa anthu ake kufunika koonetsa khalidwe limeneli . Ndipo cikristu cinayamba kufalikila ku magawo atsopano , ndipo anthu amitundu yonse analandila coonadi . ( Mac . 14 ( Yohane 15 : 20 ) Akristu a misinkhu yonse angaphunzile zambili pa cikhulupililo ndi kulimba mtima kwa Yosefe wacinyamata . CIDANI CIFIKA PACIMAKE Kuyembekezela kukapeza zabwino zokha - zokha m’cikwati ndiye kumakhalanso muzu wina wa mavuto . Mu Ufumu wa Roma , nkhondo zinacititsa kuti akhale na akapolo ambili . Nthawi zina , akapolo akacepa , anali kupita kukamenya nkhondo . KWA OKWATILANA Kodi Akristu odzozedwa ayenela kudziona bwanji ? ​ — 1 Akorinto 4 : 6 - 8 . Mwacionekele , Paulo anali kukamba zocitika za m’nthawi ya Mose kuti alimbikitse Timoteyo . Ndiponso , iye anali kukumbutsa Timoteyo kuti Yehova amadziŵa munthu akayamba kukhala ndi maganizo opanduka . Mu 1962 , tinasangalala ndi Msonkhano Wacigawo wakuti , “ Atumiki Olimba Mtima . ” Iwo akupita ku dela lina lakutali la m’dzikoli kukalalikila Makolo naonso amasamalila ana ao m’njila zosiyanasiyana . Onse anali pa mpikisano wa mbeta kuti mfumu isankhepo mmodzi . Yesu anakamba kuti uthenga wabwino udzalalikidwa mpaka mapeto . Cikumbumtima cimathandiza anthu ambili kupewa kucita zoipa . Koma kuti tiimvetse bwino mfundo yake , tiyeni tingoiganizila motele nkhaniyo . 6 : 19 ) Yesu ananenanso fanizo losonyeza mmene “ nkhawa za moyo wa m’nthawi ino ndiponso cinyengo camphamvu ca cuma ” zimalepheletsela coonadi ca Ufumu kukula . 43 : 10 ; 1 Tim . YEHOVA anali ndi colinga polenga dziko lapansi . Sara ndiye mkazi yekha amene Baibo imachula zaka zake pamene anamwalila . ( Yohane 17 : 3 ; 2 Timoteyo 3 : 16 ) M’pempheni kuti akuthandizeni kumvetsetsa Malemba . Anali ndi motoka yakale imene ananigulitsa madola 25 , ndendende ndalama imene n’nagulitsa motoka ija yowonongeka . ( Mat . 13 : 23 ; 21 : 43 ) Conco , m’fanizo limeneli , zipatso zimene Mkhristu aliyense afunika kubala sizitanthauza ophunzila atsopano amene tingapange iyai . Kukamba zoona , nimatonthozedwa kudziŵa kuti Yehova akuyembekezela moleza mtima kuti adzathetse mavuto athu na kudzatipatsa nchito yokondweletsa m’dziko latsopano . Nthawi zina tinali kuzunzidwa , koma ‘ sitinasoŵe koloŵela . ’ Pambuyo pophunzila mfundo zina za m’buku la Levitiko , kodi mukuyamikila kwambili kuti buku limeneli linalembedwa m’Baibulo ? ( 2 Tim . Limbitsani ubwenzi wanu ndi Yehova Mulungu mwa kuphunzila Baibulo ndi kupemphela nthawi zonse . ( Maliko 7 : 5 ) Apa adani amenewa sanali kutanthauza kusamba m’manja kumene tonse timacita tikafuna kudya . N’cifukwa ciani anthu ambili amapita ku maiko ena ? 3 : 8 ) Cifukwa ca zimene zinawacitikila , anthu ena othaŵa kwawo amakhala omangika , ndipo angacite manyazi kuuzako ena mavuto awo , maka - maka pakakhala ana awo . Conco , kupitila m’nsembe ya dipo , Yehova anaonetsa kuti amakonda anthu . 8 : 22 ) Kenako , anathandizila kulenga angelo ena , zinthu zakuthambo , pothela pake anthu . ( Akol . Conco , iwo anapita okha kukawatulutsa . Kodi tiphunzilapo ciani pa zimene Mulungu anacita Satana atam’pandukila ? Mwacidalilo , timayang’ana kwa “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse ” kuti atilimbikitse . ( 2 Akor . Ndiyeno imwe mufunsa wokuonetsani malo kuti , “ Kodi ici n’canyowaniko ? ” Ndiyeno Hagara anati kwa Yehova : “ Inu ndinu Mulungu amene amaona ciliconse . ” — Genesis 16 : 4 - 13 . ( b ) Kodi nkhani ya Loti ndi ana ake itiphunzitsa ciani ? Funso limeneli lakuti : “ Cili m’dzanja lakoco n’ciani ” ? 3 Ubatizo Ni Wofunika kwa Mkhristu Aliyense Akhiristu ofikapo mwauzimu angapemphe acatsopano kuti awapelekeze kukacezela odwala ndi okalamba . Mwacionekele , abalewo analibiletu ganizo logonja pa cikhulupililo cawo . ( Easily Led — A History of Propaganda ) Mwacitsanzo , pulofesa wina wa ku Britain , dzina lake Philip M . Taylor analemba kuti Asuri anali kugonjetsa adani awo mwa “ kuwaopseza ndi kufalitsa mauthenga abodza . ” 5 FUNSO : Kodi anthu onse abwino amapita kumwamba ? * Pemphani Mulungu kuti akukhululukileni , ndi kuti mukhale na cikumbumtima coyela . Panthawiyo tinali kuvina m’mabwalo ambili padziko lapansi , ndipo tinali kuvina ndi akatswili ena monga Dame Margot Fonteyn ndi Rudolf Nureyev . Conco , pofuna kuti nchito yolalikila isasokonezeke , tinali kutsatila malamulo , tili na cikhulupililo cakuti zinthu zidzasintha m’tsogolo . Usiku umenewo Yesu anawapemphelela kuti akhale ogwilizana . Iye anafotokoza kuti utumiki wa pangano latsopano ni “ cuma m’zonyamulila zoumbidwa ndi dothi . ” ( 2 Akor . 4 : 7 ; 1 Tim . 1 : 12 . ) 7 Kodi Mumafuna Kukhala Wodziŵika kwa Ndani ? M’nkhani zotsatila za m’magazini ino , mudzapezamo mfundo zothandiza zimene ziyankha mafunso amenewa . Palibe cinthu cokondweletsa kwambili kuposa kuona ophunzila Baibulo akusintha umoyo wao cifukwa codziŵa Yehova . Tingaphunzile zambili kwa aja amene anali kutumikila panthambi zimene anaphatikiza pamodzi . Posakhalitsa , Yakobo anatumiza mnyamata Yosefe paulendo . Koma cimatiŵaŵa kwambili ngati Mkhristu mnzathu kapena wacibululu wakamba kapena kucita zinthu zotikhumudwitsa . M’maiko ambili ciŵelengelo cacikulu ca amenewa ndi akazi . Pamene tikugwila nao nchitoyi , timakhala tikulalikila uthenga umodzi ndi abale athu padziko lonse lapansi mogwilizana . Baibo imayelekezelanso anthu amene amakhulupilila Yehova na ziwombankhanga . Imati : “ Anthu odalila Yehova adzapezanso mphamvu . Oliver na Anna 9 - 11 . ( a ) Fotokozani zimene tingaphunzilepo pa citsanzo ca Sebina . ( b ) Kodi imwe mwalimbikitsidwa bwanji na mmene Yehova anacitila zinthu na Sebina ? Kumbukila , colinga cako ni kuwafika pamtima anthu , osati kuwagometsa iyai . Gidiyoni anali citsanzo cabwino ngako ca kudzicepetsa . Ku Sokuluk n’kumene kunakhazikitsidwa mpingo woyamba m’dziko la Kyrgyzstan . Umu munali m’caka ca 1958 . Sonyezani kuti mumakhulupilila Yehova mwa kuika nchito yolalikila patsogolo ( Onani ndime 17 ) Komabe , Yehova angakondwele kwambili ngati mungadzipatulile kwa iye kuti mucite cifunilo cake kaamba kozindikila ubwino wa ulamulilo wake . ( Miy . Ray Bopp anati : “ Anthu pamsonkhanowo anakondwela ngako . ” 21 : 22 ; 23 : 6 ) Conco , Yehova anacita pangano ndi Abulahamu ndi mbadwa zake . ( Aroma 12 : 15 ) Kuyesetsa kukhala oleza mtima tsopano pamene tikuyembekezela kukwanilitsidwa kwa malonjezo a Yehova kudzatithandiza kuti tidzakhale oleza mtima mtsogolo . — Mlal . Ngati muleza mtima ndi kupitilizabe kukonza zinthu m’banja lanu , onse angayambenso kukukondani ndi kukulemekezani . Zikanakhala zomveka ngati iye anada nkhawa ngakhale kutaya mtima . Koma mfundo imeneyi inabutsa mafunso angapo . Mau a Mulungu amatilangiza kuti sitifunika kupupuluma popanga zosankha zofunika kwambili . 26 Lalikilani Uthenga Wabwino Wokamba za Kukoma Mtima Mau akuti “ kumwamba kwatsopano ndi dziko lapansi latsopano , ” aonetsa kuti kudzakhala boma latsopano ndi anthu abwino amene adzalamulidwa na bomalo . Ndiye cifukwa cake Baibulo limanena kuti zokamba zathu zili ndi mphamvu ya imfa ndi ya moyo . Pamene tipitiliza kukonda na kuyamikila nzelu zocokela kwa Yehova , tidzakhala okonzeka kugwila nchito yathu yophunzitsa ena mau a Mulungu . Ndiyeno mai wina wacikulile anabwela akuthamanga uku akulila , n’kumanena kuti : “ Conde alekeni . Mmenemo , timaŵelengamo mau a Yesu okamba za anthu amene anakhalabe mbeta , monga iye , “ cifukwa ca Ufumu wakumwamba . ” Kulimbitsa cikhulupililo kumafuna khama , koma Yehova adzatidalitsa ngati tiyesetsa kucita zimenezo . Caka ciliconse , mipingo yatsopano yokwana 2,000 imakhadzikitsidwa . Ndiye cifukwa cake Solomo anatiuza kuti tiyenela kukumbukila Mlengi wathu Wamkulu tikali acinyamata . — Ŵelengani Mlaliki 12 : 1 - 5 . 52 : 7 ) Mlongo wina , dzina lake Dorothy , anati : “ M’gawo lathu , ambili amaphunzitsidwa kuti Mulungu ni wankhanza komanso wokonda kupeza ena zifukwa . Mwina angaganizile mau amene Paulo anakamba kwa Akhristu a ku Korinto akuti : “ N’cifukwa ciani ufulu wanga ukulamulidwa ndi cikumbumtima ca munthu wina ? ” Sindidzitama kuti ndinasintha khalidwe langa , koma ndimakhulupilila kuti ndi umboni wakuti Baibulo lili ndi mphamvu zosintha anthu . — Aheberi 4 : 12 . Wamasalimo anaimba kuti : “ Ndiyendetseni m’njila ya malamulo anu , pakuti ndikukondwela ndi njila imeneyi . ” ( Sal . Conco , mukhoza kudela nkhawa kuti mwina mwana wanu angayambe bwino - bwino kutumikila Mulungu , koma m’kupita kwa nthawi angasinthe n’kuleka kukonda coonadi . ( b ) Kodi liu lakuti “ manda acikumbutso ” limasonyeza ciani ? Muzikumbukila Yosefe amene anagulitsidwa ku ukapolo , koma Yehova “ anamulanditsa m’masautso ake onse . ” ( Mac . Mwacitsanzo , simungayembekezele mwana wanu kuti azikamba zoona ngati amakumvelani mukamba kuti , “ Auze kuti nacokapo , ” pamene simufuna kukamba na munthu wina amene wabwela pakhomo panu . Zimene ndunayo inaphunzila zinaifika pamtima cakuti inabatizika . Ndinakhalanso tate wabwino kwa mwana wathu . Inu acicepele , muzigwilizana ndi acikulile okhulupilika a m’banja lanu ndi a mumpingo kuti mudziŵe zinthu zabwino zimene Yehova wawacitila . CIKHULUPILILO ca Mkhiristu ni khalidwe la mtengo wapatali kwambili . Panthawiyo , abale na alongo anali kulemba maadiresi a anthu amene alembetsa kuti azilandila magazini a Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani . Maadiresiwo anali kuwalemba pa tumalata tung’ono - tung’ono . Cinanso , Yesu anadzipeleka kwambili pa nchito yolalikila na kuphunzitsa anthu uthenga wabwino . M’BALE wina wacinyamata wosakwatila , amene tam’patsa dzina lakuti Eduardo , anafotokozela Stephen , mkulu wacikulile wokwatila , zinthu zimene zimamudetsa nkhawa . Delphine analemba maina a anthu ochulidwa m’Baibo amene panthawi inayake anavutika na cisoni cacikulu . N’nadzimva kuti ndine ‘ woonongekelatu . ’ ” 10 : 31 . Iwo anali kuoneka kuti ni ocita bwino mwauzimu , ndipo anali akhama mu ulaliki . Kugwila nchito yolalikila nthawi zonse kudzakuthandizani kukhala wolimba kuuzimu na kujaila mwamsanga mu mpingo watsopano . Iyi inali nthawi yoyamba , pambuyo pa zaka zambili , kumuona Peter ali wacimwemwe . N’zoona kuti timaipidwa na makhalidwe amenewa . Komabe , tingathe kutengela makhalidwe na maganizo oipa a anthu amene timakhala nawo . Mu ulosi wake wopezeka pa Mateyu caputala 24 ndi 25 , Yesu anachula za kubwela kwake mobwelezabweleza . Caka ciliconse , ana opitilila 500,000 amafa cifukwa ca matenda othulula . Nthawi zambili zimakhala cifukwa ca kusataya moyenelela zonyansa za anthu . Delalo linaphatikizapo Bulacan , Nueva Ecija , Tarlac , ndi Zambales . Satana amafuna kuti tikhale akapolo a Cuma m’malo motumikila Yehova . Anthu amene amadalila sayansi kuti iwathandize kudziŵa ngati zamoyo zinacita kulengedwa , amasoceletsedwa na mfundo zosamvetsetseka za asayansi . Nditapita kumeneko , anandisonyeza zithunzi zao za pa cikwati , inenso ndinam’sonyeza zathu . Nanga n’zinthu zabwino ziti zimene nimacita ? Atumwi amenewo “ anayamba kuika manja ao pa anthuwo , ndipo analandila mzimu woyela . ” Koma limakamba kuti Luka anatumiza moni kwa Akristu a ku Kolose kupitila mwa Paulo . Ciwelewele cimacititsa mavuto aakulu ndi ozunza kwambili . Koma anthu paokha sangakwanitse kudziŵa cabwino na coipa . Kwa zaka zambili pambuyo pophunzila coonadi , Victoria zinali kumuvuta kukhulupilila kuti Mulungu amam’konda . Ngakhale masiku ano , alipo acinyamata amene amayamikila zinthu zauzimu . Pamenepa Mulungu anaonetsa m’njila yapadela kwambili kuti anayamikila utumiki wokhulupilika wa Yesu . ( Aroma 6 : 14 ) Conco , tili pansi pa ulamulilo wa kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . Kamasulidwe katsopanoka n’kogwilizana kwambili na tanthauzo la mau a Ciheberi ndi kalembedwe ka citundu cimeneci . ( Aroma 2 : 11 ; Agalatiya 3 : 28 ) Nkhani ya Debora imatikumbutsa kuti Yehova amadalitsa akazi ndi mwai wautumiki ndipo amawakonda ndi kuwakhulupilila . Banja lingasinthe zinthu zina n’colinga cakuti lisamaononge ndalama zambili kuposa zimene limapeza . ( Yes . 65 : 21 , 22 ) Sikudzakhala kupondelezana , umphawi ndi njala . ( Sal . Petersburg . Rachel , amene tamugwila mau poyamba anavomeleza zimenezi . Mungaonenso Genesis 1 : 2 ; ndi Machitidwe 2 : 1 - 4 ; 10 : 38 . Limatiuzanso kuti tiyenela kukhala oganiza bwino pa zinthu zimene timacita monga kudya ndi kumwa . Popeza kuti Goliyati anali wamtali mikono 6 ndi cikhatho cimodzi , ndiye kuti anali wamtali mamita 2.9 . Pamene wapolisi anali kunifunsa mafunso m’ndende , ananizazila , amvekele : “ Posacedwapa tidzakuphwanyani monga nsabwe ! ” Mwana wa Yefita analola kukhala wosakwatiwa ndiponso kusakhala ndi ana kuti atumikile Yehova N’zosadabwitsa kuti asilikali ambili anagalukila atsogoleli ao . ( 1 Akor . 8 : 3 ) Conco , nthawi zonse muziyamikila mwayi wamtengo wapatali umene muli nawo wokhala m’gulu la Yehova . 3 : 13 ) Kumwamba kwakale ndi dziko lakale zikutanthauza maboma oipa ndi anthu oipa amene amalamulidwa ndi mabomawo . Koma nkhani imeneyi munalibe m’magazini ya Cijelemani . Yehova analonjezelatu kuti adzaika pamodzi ndodo ziŵilizi kuti zikhale ndodo imodzi m’dzanja lake . ( Ezek . 4 : 7 , 8 ) Komabe , ngati Mulungu wakupatsani ciyembekezo cina , sindiye kuti wacita zinthu mopanda cilungamo . Ngakhale n’conco , banjali linali kukumanabe na mavuto a m’dzikoli . Kupyolela mwa Mose , Yehova anacita pangano lapadela ndi mtundu umenewu mwa kuwapatsa Cilamulo . Ndipo mtundu wa Isiraeli unavomeleza zonse zokhudza pangano limenelo . 1 : 6 ; 2 Pet . Nthawi ikubwela pamene munthu aliyense adzakhala ndi zonse zofunikila monga cakudya copatsa thanzi ndi nyumba yabwino . AFILIPI 1 : 10 , 11 Mwa kupeleka Mwana wake wobadwa yekha , Yesu Khristu monga dipo , Yehova Mulungu anapeleka ciyembekezo ca moyo wosatha kwa anthu omvela . Koma sikuti colinga ca Yesu cinali cofuna kuwononga cibululu ca anthu . Colinga cake cinali kulengeza uthenga wa Mulungu wonena za coonadi . ( Yoh . Adamu sanangotaya cabe tsogolo lake labwino , koma anapatsilanso ana ake kupanda ungwilo , ucimo , na imfa . Kucita zinthu mwanjila imeneyi nafenso kungatithandize . — 1 Akor . Ngati n’kotheka , ŵelengani ngakhale lemba limodzi pokambilana ndi mwininyumba . Kodi mudzayesetsa kuona zabwino mwa m’baleyo ndi kuganizila zaka zambili zimene iye watumikila Mulungu mokhulupilika ? Mlongoyu anati : “ Ngati Kingsley wakwanitsa inenso ndingakwanitse . ” “ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi maganizo ako onse . ” — MAT . Mudzamvetsa malamulo ake ndi kuona mmene anacitila zinthu ndi anthu ake akale . Komabe , Yesu anakamba kuti anthu ambili ‘ adzanyalanyaza ’ kapena kuti sadzadziŵa za kukhalapo kwake , ndi kuti adzatangwanika ndi zocitika za paumoyo mpaka zinthu zitafika pa mwana wakana phala . Anthu ena amaona nchito yoyeletsa kukhala yofunika kwambili kuposa mmene ena amaionela . Kuti zimenezi zitheke , tifunika kugwilitsila nchito nzelu zothandiza , kukhulupilila Mulungu , ndi kukhala ndi ciyembekezo ceniceni ca mtsogolo . Kuwonjezela apo , mumayesetsa kupewa kutangwanika na zinthu za m’dzikoli . Kumeneko , atsogoleli a cipembedzo anatuntha acicepele kuti ayambe kuponya miyala pa nyumba ya amishonale imene tinali kukhala , imenenso inali yowonongeka kale . Tiyamikila kwambili kuti Yehova anatipatsa cikumbumtima . 25 : 8 , 15 , 16 ) Panali pomveka Davide kupempha thandizo kwa Nabala cifukwa iye ndi anyamata ake anateteza cuma ca Nabalayo . A Yohane : Tidzaonana , ndipo ine ndi mkazi wanga tidzaŵelenga nkhaniyi pamodzi . Anthu amene ali pa ubwenzi amalankhulana nthawi zonse kuti alimbitse ubwenzi wao . ( Sal . 12 : 8 ) Khalidweli lafala kwambili cakuti mungadzifunse kuti , ‘ Kodi n’zothekadi kukhala wodziletsa ? ’ Pocoka ku Africa tinali ndi nkhawa kwambili kuposa pocoka ku America . ( Yer . 17 : 9 ) Ngati mwaona kuti penapake zinthu sizinayende bwino , pemphani mzimu woyela kuti ukutsogoleleni . Cifukwa ca matenda oopsa amenewa , Jairo anafunikila kumamucitila zinthu zonse monga kumudyetsa , kumuveka , komanso kumugoneka . Mavuto amene angakumane nao cifukwa ca khalidwe lake loipa , ndiponso kukumbukila mmene anali kusangalalila pamene anali pa ubwenzi wabwino ndi Yehova ndi anthu ake , zingamuthandize kuzindikila kulakwa kwake . 19 : 8 ) Koma n’zacisoni kuti m’kupita kwa nthawi , mtunduwo unalephela kuseŵenzetsa bwino ufulu wawo , ndipo unaphwanya lonjezo lawo limenelo . 8 : 56 ) N’cimodzi - modzi na Sara , Isaki , Yakobo ndi ena ambili . Iwo anaika maganizo awo pa Ufumu wa kutsogolo , “ umene Mulungu ndiye anaumanga ndi kuupanga . ” — Aheb . Yehova Mulungu anamvela cisoni cifukwa ca masautso amene Aisiraeli anakumana nawo mu ukapolo ku Iguputo . Iye amamvelanso cimodzi - modzi akaona zinthu zopanda cilungamo masiku ano . Sikuti iye amangofuna cabe kuteteza atumiki ake ku mavuto amene angakumane nao cifukwa cosankha zinthu mopanda nzelu , koma amafunanso kuti tikhale osangalala . Conco , sayenela kuona kuti lipoti la utumiki wao n’losafunika . Kodi gulu lathu limacita bwanji kuti zopeleka zizigwilitsidwa nchito moyenela ? Mpingo wina ku Istanbul unalemba kuti : “ Anthu akationa , anali kutifunsa kuti : ‘ Kodi kuli msonkhano wapadela ? Wonyenga iwe ! NYIMBO : 72 , 124 N’nali mmodzi wa ana 7 , ndipo pamene n’nali mnyamata n’naphunzila nchito zambili zaulimi Conco , n’zomveka kuti Paulo anali kukamba za nkhani ya pa Numeri 16 : 5 , 23 - 27 pamene analemba kuti : “ Aliyense wochula dzina la Yehova aleke kucita zosalungama . ” Cinanso , zioneka kuti ma IUD okhala na kopa akaikidwa m’cibalilo , kopayo imapha mbeu ya mwamuna . Zocitika zimenezi zimatikumbutsa mau a Yesu akuti : “ Odala ndi anthu amene amazindikila zosoŵa zao zauzimu . ” Inde , Paulo anali kukonda kupeleka moni kwa abale na alongo ake . — Aroma 16 : 1 - 16 . ( Agalatiya 4 : 13 ) Izi zigwilizana ndi zimene Yesu anakamba kuti “ odwala ” amafuna dokotala . — Luka 5 : 31 . M’bale wina wa ku India , amene ali na famu ya makokonati , anapeleka makokonati ambili ku ofesi yomasulila mabuku ya Cimalayalam , monga copeleka caufulu . Anaona kuti ni bwino kupeleka makokonati kusiyana ndi kupeleka ndalama , cifukwa pa ofesiyo abale amafunika kugula makokonati . ( Genesis 41 : 33 - 36 ) Yosefe anali wa luso ndi wodziŵa zinthu kwambili , ndipo ndiye anali woyenela kugwila nchito imeneyo . Pamene ndinafotokozela anzanga zimene zinacitika , mmodzi wa akulu anandifunsa kuti : “ M’bale Stephen , ukanaigwila , ukanaicita ciani ? ” Paulo anakamba kuti : “ Cotelo , popeza kuti tili ndi mphatso zosiyana - siyana mogwilizana ndi kukoma mtima kwakukulu kumene tinapatsidwa , . . . ngati tili ndi mphatso ya utumiki , tiyeni ticitebe utumikiwo . Amene akuphunzitsa , aziphunzitsa ndithu . Wocenjeza , aike mtima wake pa kucenjeza . . . . Wotsogolela , atsogolele mwakhama . Ndipo wosonyeza cifundo , acite zimenezo mokondwa . ” Nanga iwo n’ndani ? Yaciŵili idzationetsa mmene tingakhalilebe odzicepetsa pa mayeselo . ( Ŵelengani Maliko 12 : 30 . ) Pa zocitika zonse , tifunika kudalila Yehova kuti atitsogolele . Tizikhulupilila kuti adzaticilikiza pa zimene tiyenela kucita , ndipo adzaticitila zimene sitingakwanitse . Kukambilana zimenezi kutilimbikitsa kutsatila malangizo a Yehova otsogolela ku moyo wosatha . Komanso kucita zimenezo kukanaika moyo wa Natani paciopsezo . ( 2 Pet . 3 : 13 ) Nzika zonse za dziko latsopano limenelo zidzayenela kutsatila miyezo ya Yehova . — Yes . 3 : 17 . Komabe , mipingo yambili ikali kufunika thandizo . Mukalibe kusankha njila iliyonse , muyenela kufunsa ku ofesi ya nthambi kuti mudziŵe njila zimene ndi zotheka m’dziko lanu . Kunena zoona ndinali kufunikila kupanga masinthidwe aakulu , makamaka umunthu wanga . Iye anati : “ Ndine wamng’ono kwambili mwa atumwi onse , ndipo si ine woyenela kuchedwa mtumwi , cifukwa ndinazunza mpingo wa Mulungu . ” N’ciani cingatithandize kuti tiziona nchito moyenelela ? Zoona , sitingakaikile za zimenezi . Koma patapita zaka zambili ndinayamba kukoka ndudu zambili . Conco pemphani Mwini zokololazo kuti atumize anchito okam’kololela . ” Nkhani za m’magazini ino zifotokoza nkhani yocititsa cidwi ya mmene Baibulo yapulumukila . ( Aroma 15 : 5 ) Mzimu woyela ungatithandizenso kuzula zilakolako za thupi ndi kukulitsa makhalidwe okondweletsa Mulungu . ( Agal . ( Luka 10 : 33 - 37 ) Njila yabwino kwambili imene tingawathandizile ndi kuwauzako uthenga wabwino . Wosimba ndi William Samuelsoan Mabanja ena amacita maseŵelo a nkhani za m’Baibulo . Koposa zonse , muzigwila mokhulupilika nchito iliyonse imene mwapatsidwa . Kuseŵenzetsa mfundo za m’Baibo na kupempha mzimu wa Mulungu kudzatithandiza kupeza mtendele Tili ndi mwayi wothandiza anthu ofuna - funa coonadi kudziŵa yankho la funso lofunika kwambili limeneli pamene tiwaitanila ku Cikumbutso , pamene tipezeka pa Cikumbutso , ndi pamene tibwelelako kwa iwo . Conco , iwo akanasangalala ndi zinthu zambili zokongola m’mudzi wawo wa Paradaiso . NYIMBO : 39 , 77 Pamene ndinali kutumikila kumalo osowa , ndinasangalala kuona ophunzila Baibulo anga akubatizidwa . N’cifukwa ciani tifunika kusankha mabwenzi athu mwanzelu ? Atumwiwo anamuthaŵa . Ngati ndinu kholo , mwacionekele mukumvetsa mmene Manowa anamvelela . Komabe , yankho la funso limeneli lipezeka m’macaputala aŵili oyambilila a Genesis , buku loyamba m’Baibulo . Iye anati : “ Nikalibe kukhala Mboni , n’nali kuseŵenza pa kampani ina yaikulu . Mwiniwake wa kampaniyo anali kucitila lipoti ndalama zocepa monga phindu la kampaniyo kuti azilipila msonkho wocepa . Tiyeni tikambilane citsanzo cimodzi . Nthawi zonse , iye amayesa kukupangitsani kukayikila anthu amene Yehova wawaika kuti azikutsogolelani . Mayi wina wa zaka za m’ma 50 , dzina lake Eunice , anakamba kuti : “ Baibo ikunithandiza kukhala munthu wabwino , ndiponso kusintha zizoloŵezi zanga zoipa . ” Ndiyeno io anakambitsilana zoonjezeleka zokhudza Mulungu woona . Timafika podziŵa kwambili umunthu wao ndi makhalidwe ao . Iye ananena kuti nchito inali kuyenda bwino m’kafiteliya cifukwa ca cikondi . Sikuti anthu amene amacita utumikiwu ni apadela , koma utumiki wawo ndiwo wapadela . Iwo amadziŵa kuti afunika kuyesetsa kusunga lonjezo lawo pamene ali mu utumiki wanthawi zonse wapadela . Pelekani citsanzo cimene cionetsa mmene Yesu anali kuonela akazi . Panyumba pathu tinali ndi Korani , Tora , ndi Baibulo . Imfa ya Yesu ndi yapadela kwambili m’mbili ya anthu . 12 , 13 . ( a ) N’cifukwa ciani nthawi zina Akhristu amasemphana maganizo ? 24 Yehova Amapeleka Mphoto kwa Anthu Omufuna - funa na Mtima Wonse Zaka zimenezi n’zoculuka kuposa zaka za anthu anayi okalamba ngako masiku ano . KHALANI WOPATSA : “ Khalani opatsa ndipo inunso anthu adzakupatsani . ” Baibulo limati : “ Anthu amene amamuopa adzawacitila zokhumba zao , adzamva kufuula kwao kopempha thandizo ndipo adzawapulumutsa . ” Mu 1976 , tinaitanidwa kukatumikila ku ofesi ya nthambi ya ku Austria m’tauni ya Vienna . Iwo amakhulupilila Mulungu amene analonjeza kuti : “ Sindidzakusiyani kapena kukutayani ngakhale pang’ono . ” N’kutheka kuti ali na cikhulupililo colimba , ni opilila , opanda mantha , kapena ali na makhalidwe enanso abwino . Kuganizila zimenezi kudzacititsa kuti tiziwakonda kwambili , ndipo kudzatilimbikitsa kuwaceleza na mtima wonse . Mofananamo , akulu masiku ano afunika kutengela citsanzo ca Yohane mwa kulimbikitsa abale na alongo kuti ‘ asafooke . ’ — Yes . Tifunika kupewa zosangalatsa zoipa zimene zingatilepheletse kuikabe maganizo athu pa mphoto ya moyo . — Miy . N’namvela monga mtima wanga wang’ambika . Kukhalapo kwathu komanso kwa cilengedwe conse ndi umboni wakuti kuli Mulungu wamuyaya . PACIKUTO : M’bale wacinyamata akucita ulaliki wamwai ndipo akuonetsa munthu wina vidiyo pa jw.org mu mzinda wa Esperanza Kodi Baibo yathandiza bwanji anthu kusintha umunthu wawo ? Masiku ano kuposa kale lonse , akatswili a Baibo ndiwo ali pa malo oyenelela opendanso ma Baibo ena akale . Ponena za wolamulila wamtsogolo , ulosiwo umati : “ Anamupatsa ulamulilo , ulemelelo , ndi ufumu kuti anthu a mitundu yosiyanasiyana azimutumikila . Atumiki ena a Yehova , monga wophunzila Sitefano ndi ena , anaphedwa cifukwa ca kukhulupilika kwao . N’cifukwa ciani tiyenela kupatula nthawi yophunzila Baibulo ndi kucita Kulambila kwa Pabanja mlungu uliwonse ? Mwacitsanzo , kodi mwana wanu amatsutsa ziphunzitso za m’Baibulo ? Kapena amangocita mantha kulalikila anzake ? Tikamaliza kuliona , tinali kulitumizanso ku nthambi kuti likasindikizidwe . Zikomo kwambili Yehova . ” Ngati ndi kapepala kakuti Kodi N’zoona Kuti Akufa Angakhalenso ndi Moyo ? , tingafunse kuti : “ N’cifukwa ciani timakalamba ndi kufa ? ” ( Salimo 36 : 9 ) Pokamba za iye , Yesu Khristu anapemphela kuti : “ Pakuti moyo wosatha adzaupeza akamaphunzila ndi kudziŵa za inu , Mulungu yekhayo amene ali woona , ndi za Yesu Khristu , amene inu munamutuma . ” ( a ) Tingapindule bwanji ndi mafanizo aŵiliwa ? Kundendeko anatiikanso pamodzi ndi akaidi ena amene sanali a Mboni . M’bale Jensen anakamba kuti nchito ya manja inganithandize kukhala wathanzi . Yehova anapeleka munthu wangwilo kuti akhale dipo . Kodi Kumva Cisoni n’Kulakwa ? ( b ) Kodi mwatsimikiza mtima kucita ciani pankhani ya kukhalabe woyela ? M’fanizoli , mbuye anayamikila kapolo aliyense na mau akuti : “ Wacita bwino kwambili , kapolo wabwino ndi wokhulupilika iwe ! Panthawi imene mudzazindikila kuti ciswe cadya nyumba ndi m’mbuyo mwa alendo n’kuti nyumbayo ili pafupi kugwa . Malemba amatiuza kuti “ Abulahamu ataonetsa kuleza mtima , ” analandila lonjezo lakuti Yehova adzamudalitsa na kuculukitsa mbadwa zake . ( Aheb . Kodi inuyo mungakwanitse kukathandiza pa nchito yokolola mwa kusamukila kumalo amene kukufunika ofalitsa Ufumu ambili ? Kodi zimene Mwiitiyopiya wotembenukila ku Ciyuda ndi mtumwi Paulo anacita zitiphunzitsa ciani ponena za ubatizo ? Umenewo ndi ulosi wolembedwa mu Danieli caputala 4 . Corinna anati : “ Tinacoka m’madzulo kumene tinali kuseŵenzela ndi kupita ku sitesheni ya sitima imene inali pa mtunda wa makilomita 25 . Kodi Mkhristu wodzipeleka wobatizika afunika kuzindikila ciani ? Bwanji osaliŵelenga ndi kuona mmene lingakuthandizileni inuyo panokha ? Dikishonale ina inamasulila kunyadila kuti ndi : “ Kukhala wokhutila cifukwa ca zimene mwacita , zimene muli nazo , kapena cifukwa ca zimene mnzanu wacita ndiponso zimene ali nazo . ” Muzipeleka cilango coyenelela . N’zoona kuti aliyense amafuna kugula zovala za kumtima kwake malinga ndi thumba lake . Cihema ca Mulungu cili pakati pa anthu . . . . Iye adzapukuta misozi yonse m’maso mwawo , ndipo imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . ( Luka 18 : 4 , 5 ) Ngati woweluza wosalungamayo anathandiza mkazi wamasiye ameneyo cifukwa coopa kuti dzina lake lingacitidwe citonzo , kodi Mulungu wacifundo sangawacitile mwacilungamo anthu “ amene amafuulila kwa iye usana ndi usiku ? ” Ndipo ngati tikukumana ndi mavuto m’cikwati , tiyenela kuonetsa kuti timakonda Yehova mwa kukhalabe okhulupilika kwa mwamuna kapena mkazi wathu . — Ŵelengani Malaki 2 : 13 - 16 . Pambuyo popezeka pa misonkhano maulendo angapo , mpainiya wina wacikulile , M’bale Damian Santos , amene kale anali meya , ananipempha kuti nikagone ku nyumba kwawo . Iye sanaganize kuti kumanga nyumbayo pamcenga kudzakhala kochipa ndipo sikudzatenga nthawi . Timaŵelenga kuti iye “ anamvela mau a [ Sara ] . ” — Genesis 16 : 1 - 3 . Mofananamo , mufunika kuyesetsa kukhala munthu wauzimu kuti mukulitse cimwemwe canu . Anali wofunitsitsa kugwilako nawo nchitoyo akapeza mpata . Ulamulilo wa Yehova si wopondeleza koma ni wololela . Tikamapemphela , Mulungu safuna kuti tizigwilitsila nchito mau odzionetsela kapena kumangobweleza mapemphelo oloweza . N’zoona kuti cilango ca Yehova cimaonetsa kuti iye amazonda chimo . Koma cimaonetsanso kuti amadela nkhawa munthu amene wacimwa . Mukamaŵelenga Baibulo , muziima pang’ono ndi kudzifunsa kuti : ‘ Kodi zimenezi zindiphunzitsa ciani ponena za Yehova ? 127 : 1 . Koma Yesu anapeleka moyo wake monga nsembe pafupifupi zaka 2,000 zapitazo . N’ciani cingacitike ngati sindinagwile nchitoyi kapena ngati sindinaigwile moyenela ? Satana ndi dziko lake akuyesetsa kutifooketsa ndi kuticititsa kuti tisamaone cuma cauzimu cimene taphunzila m’nkhani ino kukhala cofunika . Kuti moyo woyamba upitilize , unafunikila kubala wina — winanso kubala unzake , ndi kupitiliza conco . Iye anapemphela kwa Yehova kuti amuthandize cifukwa analibe ndalama zokwanila ndi malo ogona . Dziko la Satanali lacititsa kuti anthu avutike kwa zaka zoposa 6,000 , koma posacedwapa lidzawonongedwa . TSAMBA 11 • NYIMBO : 114 , 101 Conco , Mulungu anali kudzabweletsa cigumula padziko lapansi cimene cinali kudzaononga anthu oipa . — Gen . Kodi Davide analidi mwana ? Wathyola uta ndi kuduladula mkondo . Ndipo watentha magaleta pamoto . ” — Salimo 46 : 8 , 9 . 14 , 15 . ( a ) Kodi Zekariya anaona ciani m’masomphenya ake a namba 7 ? ( 1 Akor . 6 : 9 - 11 ) Inde , N’zokondweletsa kuona mmene Mulungu amathandizila anthu a ‘ maganizo abwino amene adzapeza moyo wosatha ’ kusintha ndi kukhala paubwenzi ndi iye . ( Mac . Ndiyeno , ife ndi Mboni zina tinakakamizidwa kubwelelanso ku Malawi kumene anali kutizunza . Ndipo tizikumbukila kuti : Amene adzalandila mphoto ndi aja amene amapilila . Musanayankhe funso imeneyi , ganizilani mwambi uwu umene umati : “ Mau onenedwa pa nthawi yoyenela ndi abwino kwambili . ” — Miy . Tsopano , iye amakudziŵani . Wosimba ni Andreas Golec Timapindula bwanji na malangizo amene Yehova amapeleka kupitila mwa “ mtumiki woyang’anila nyumba wokhulupilika ” ? Siniiŵala zithunzi - thunzi zimenezo . ” ( Yes . Zolinga sizili monga maloto cabe amene ungakonde kuti acitike . N’cifukwa cake iye alibe ufulu wolamulila cilengedwe . 40 : 8 . Ndithudi ayi ! Nthawi yabwino imene munthu angakhale na makhalidwe amenewa ni pamene ali wamng’ono . Kumapeto kwa seŵelo limeneli , anali kuonetsa mtendele umene udzakhalako Yesu Kristu akadzayamba kulamulila dzikoli . 15 Kodi Mumasankha Bwanji Zocita ? Izi n’zimenenso ana anu angacite ngati mumangowapatsa macenjezo akabwela kwa inu kupempha nzelu . Iye anakaikila ngati anthu amatumikila Mulungu ndi mtima wonse . ( Ezek . 14 : 14 ) N’cimodzi - modzinso na atumiki a Mulungu masiku ano . Komabe , tonse tifunika kuvala zovala zimene zingathandize ena kusunga ciyelo cathu ca m’maganizo , m’mau , ndi m’zocita zathu . Analibenso zida zankhondo zomenyela adani awo kapena zodzitetezela . Koma adani awo anali ndi magaleta ankhondo 900 okhala ndi zitsulo zazitali zakuthwa m’mawilo . — Ower . Lomba tiyeni tikambilane mayankho pa mafunso atatu ofunika aya : ( 1 ) Kodi cilango ca Mulungu cimaonetsa bwanji kuti amatikonda ? Nkhani ziŵilizi zidzafotokoza tanthauzo la ufulu weni - weni , mmene tingaupezele , na mmene tingaseŵenzetsele ufulu wokhala na malile umene tili nawo , kuti tipindule mu umoyo wathu na kupindulitsanso ena . “ Elizabeti atamva moni wa Mariya , khanda limene linali m’mimba mwakemo linadumpha . Ndipo Elizabeti anadzazidwa ndi mzimu woyela . ” — Luka 1 : 41 . Timalimbitsanso cikhulupililo cathu ngati tilalikila ndi kuphunzitsa ena uthenga wabwino wocokela m’Baibulo . Masiku ano , m’gulu lathu muli zitsanzo zolimbikitsa za abale na alongo amene anakhalabe na cimwemwe pamene anakumana ndi mavuto . N’zodziŵikilatu kuti mnyamatayo sanapite kumeneko kuti akacite ciwelewele . Patangopita miyezi yocepa , n’nayamba kuseŵenzela m’Dipatimenti Yotumiza Mabuku . Iwo anali ndi ciyembekezo cabwino kwambili . Mwezi uliwonse , maulaliki a citsanzo amapezeka mu Utumiki Wathu wa Ufumu . Yesani kuwagwilitsila nchito . Timadziŵa kuti iye ndi Munthu wotani , zimene amakonda , ndi zimene sakonda . ▪ Kodi ‘ Mudzakhalabe Maso ’ ? ( a ) Kodi mau a Yesu opezeka pa Maliko 12 : 29 , 30 angagwilitsidwe nchito bwanji pokambilana ndi wophunzila ? Mtundu wa Isiraeli sunali kanthu poyelekezela ndi Ufumu wa Roma umene unali wochuka . Timaona dzanja la Mulungu pa umoyo wathu ngati tizindikila mmene iye amayankhila mapemphelo athu , ndi mmene amatithandizila Nanga ufulu umenewu tingauseŵenzetse bwanji mwanzelu ? Koma m’zaka zimenezo , anthu wamba ambili sanali kumva Cilatini . Sitileka kufuna - funa anthu a maganizo oyenela amene angawathandize kukapeza moyo wosatha Kungokhala mbali ya mpingo sikunali kokwanila monga mmene kungochula dzina la Yehova sikunali kokwanila m’nthawi ya Mose . 6 : 33 ) Mu April 1998 , Paul na Stephany anaitanidwa ku Sukulu ya Giliyadi ya namba 105 . Atatsiliza maphunzilo amenewo anatumidwa kukatumikila ku Malawi mu Africa . Mwa kugwilitsila nchito zimene zili pa kamutu kakuti “ Mmene Mulungu Adzakwanilitsila Cifunilo Cake , ” mu nkhani yapita , fotokozani . . . Koma kamasulidwe katsopanoka n’kozikidwa pa mfundo izi : Pamene Abulahamu anali kuyembekezela , kodi anataya mtima potumikila Yehova ? Conco , tikathandiza ena — maka - maka amene sangakwanitse kutibwezela — pamakhala mphoto yake . Mofanana ndi zimenezi , Davide anadziŵa kuti munthu wolungama nthawi zina amafunika kupatsidwa uphungu wamphamvu kuti asinthe khalidwe lake . N’cifukwa ciani anthu ambili sazindikila kuti zinthu zikuipila - ipila ? 6 : 1 ; 2 Tim . Iwo ndi anthu a Mulungu ! Nanga n’ciani cathandiza abale ndi alongo acangu amenewa kupitiliza kutumikila ku maiko ena ? 37 : 25 ) Dziŵani kuti Yehova amaona kuti ndinu wamtengo wapatali , ndipo ndi ‘ dzanja lake lamanja lacilungamo , ’ adzakuthandizani kupeza zonse zofunikila kuti mupitilize kum’tumikila . ( 1 Timoteyo 5 : 17 ) Sitiyenela kulemekeza odzozedwa mopambanitsa cifukwa kucita zimenezi kungawacititse manyazi . Iye amadziŵa kuti zimenezi zimatipatsa cimwemwe ceniceni . Mosasamala kanthu za mavuto amene ophunzilawo anakumana nao , uthenga wabwino “ unalalikidwa m’cilengedwe conse ca pansi pa thambo , ” pa zaka 30 cabe , ndipo ‘ unabala zipatso ndi kuwonjezeka m’dziko lonse . ’ NYIMBO : 124 , 79 Pamenepo Yehova anakhala ‘ Woweluza wao , Wowapatsa Malamulo , ndi Mfumu yao . ’ N’ciani cimene mkulu angacite asanaphunzitse m’bale maluso enaake ? N’zoonekelatu kuti Yehova amakondwela ngati tiseŵenzetsa nthawi na mphamvu zathu popititsa patsogolo zinthu za Ufumu na pothandiza okhulupilila anzathu . Ndipo ena mwa alaliki a Ufumu akhama amenewa ndi Mboni zocokela kumaiko ena zimene zinapita ku Russia kuti zikathandize pa nchito yokolola . ( Mat . Kucita zimenezi kungathandize okhulupilila anzathu kukhala omasuka . — Miy . Ndipo nthawi zambili amasiila ndani udindo wosamalila ana ? Yehova safuna kuti atumiki ake azisoŵa cakudya . Koma kubwelela n’kofunika cifukwa ngakhale kumwamba kudzakhala cisangalalo ngati ocimwawo angabwelele . — Luka 15 : 7 . Koma tsopano , ine na mkazi wanga ndife acikulile kwambili kuposa onse m’banja lathu la Beteli . Mosiyana ndi anthu odzikuza amene amakana kukhala omvela , Yesu modzicepetsa anagonjela kucita cifunilo ca Mulungu ndipo anakhala “ womvela mpaka imfa . ” Mkati mwa zaka zosaŵelengeka zimene Mulungu anali kulenga cilengedwe conse , Yesu anali pambali pake kugwila naye nchito . Ngakhale kuti ndife opanda ungwilo , tikhoza kukhala paubwenzi ndi Yehova ndiponso kum’tumikila . Koma io anakana kutengela umoyo wa kumeneko . ( 1 Mbiri 16 : 7 , 27 ) Komanso wamasalimo wina , dzina lake Etani , analemba kuti : “ Odala ndi anthu amene amafuula mosangalala . Ŵelengani Genesis 40 : 14 , 15 . Komabe , lembali limachula mwacindunji “ madzi ” omwe ndi ofunika kwambili kwa zamoyo zokhala pa pulaneti limeneli . Mwina ndinali kukhala wolema kwambili kuti ndimvetsele kapena sindinali kufuna cabe kumvetsela . Iye amaona mmene tivutikila ndipo ‘ pakuti amatidela nkhawa , ’ adzaonetsetsa kuti tiyesedwa “ kwa kanthawi ” cabe . Adamu anapatsa nyama iliyonse dzina loyenelela . Palinso mfundo zina zimene tingaphunzilepo pa zimene zinacitika Aisiraeli atangotuluka mu Iguputo . ( 1 Mbiri 28 : 9 ) Mosiyana ndi Asa , Amaziya sanali wodzipeleka ndi mtima wonse kwa Yehova . Kodi tingacite ciani kuti tipindule na lonjezo limeneli la Mulungu ? Kodi tikuyembekezela kudzasangalala ndi zinthu ziti zakuuzimu m’dziko la tsopano ? Masiku ano , anthu ambili amakhutila ndi nchito imene agwila kokha ngati anzao awatamanda cifukwa ca nchitoyo . Yehova anatilenga m’njila yakuti tizitha kutengela citsanzo cake . Imeneyi ndi njila ina imene waonetsela kuti amatikonda . Onse avala bwino . Conco , lingaphonyetse mbali zina zokhudza ziphunzitso zathu kapena citsogolo ca gulu . Komabe , iye amakhumudwa ngati timalekelela maganizo oipa kuzika mizu m’mitima mwathu m’malo mowacotsa . ( Gen . Ndipo n’nali kudzimva ngati wolephela . Mwacitsanzo , panthawi ya Cilamulo ca Mose , kunali “ akazi otumikila , amene anali kutumikila mwadongosolo pacipata ca cihema cokumanako . ” ( Eks . Mulimonse mmene zilili , mau a Yeremiya onena za kulila kwa Rakele , ndi ulosi wokamba za nthawi pamene anthu anacita ciwembu kuti aphe Yesu pamene anali mwana . Mogwilizana ndi zimene wamasalimo analemba , Yehova anati : “ Popeza [ wolambila woona ] wasonyeza kuti amandikonda , Inenso ndidzamupulumutsa . Kodi tiyenela kucita ciani ? 3 : 9 - 13 ) Ndiyeno , Mulungu anapeleka ciweluzo kwa ocimwawo . Kodi mwaona kuti cozizwitsa comaliza cimene Eliya anacita ndiye cinali cozizwitsa coyamba cimene Elisa anacita ? Ndinaŵelenga mabuku onsewo m’kanthawi kocepa cabe , ndipo ndinafuna kudziŵa zambili . Ngakhale zinali conco , Gwen anali kundithandiza , ndipo sitinaphonyepo misonkhano , kapena kupita mu ulaliki ndi ana athu m’mawa uliwonse pa Sondo tikatsiliza kukama mkaka ku ng’ombe . ( 2 Akor . 6 : 14 ) Baibulo limalangiza atumiki a Mulungu kuti ayenela kukwatila kapena kukwatiwa kokha “ mwa Ambuye , ” kutanthauza kuti ayenela kupeza Mboni yodzipeleka ndi yobatizidwa imene imatsatila ziphunzitso za m’Malemba . ( 1 Akor . Ratana wa ku India anayamba cibwenzi ndi mnyamata amene anali naye kalasi imodzi yemwenso anali atayamba kuphunzila Baibulo . ( 1 Akor . 13 : 7 ) Ngati mwaona zizindikilo zakuti wa m’banja lanu wocotsedwa wayamba kusintha , mungamupemphelele kuti apeze mphamvu kucokela m’Malemba , ndi kuti alabadile ciitano ca Yehova cakuti : “ Bwelela kwa ine . ” — Yes . KODI MUNGAYANKHE BWANJI ? Kodi tingaonetse bwanji khalidwe lopambana kwa munthu aliyense amene takumana naye mu ulaliki ? Tiyenela kucitanji tikakumana ndi ampatuko ? Nanga n’cifukwa ciani Yehova amachedwa “ Atate ” kwa Akristu amene ali ndi ciyembekezo cokhala pa dziko lapansi ? Mosiyana ndi munthu wakuthupi , munthu wauzimu amakonda kucita zimene Mulungu amafuna . Koma mzela wobadwila wa Mesiya unapitila mwa Davide . ( 1 Sam . Kumatithandiza kukhala olimba ngakhale pamene takumana ndi ciyeso coopsa kwambili . Mulungu ndi amene anawasankha kuti akakhale kumwamba . M’caka ca 1919 , wotsogolela utumiki anaikidwa mumpingo uliwonse kuti azitsogolela pa nchito yolalikila . Iwo amakumana mwacinsinsi kuti akambilane zocitila ciwembu anthu anu . ( Maliko 13 : 37 ) Yesu amafuna kuti ophunzila ake onse azikhala okonzeka komanso kukhala maso . Cimwemwe cimatanthauza kukhala na mtendele wamumtima umene umakhalapo nthaŵi zonse . Munthu wacimwemwe amakhala wokhutila mumtima , komanso wosangalala , ndipo mwacibadwa amalaka - laka kuti mtendele wamumtima upitilize . 11 : 3 ) Kodi tingaonetse bwanji kuti ciyembekezo cathu n’camoyo , ndi kuti timakhulupililadi zinthu zosaoneka zochulidwa m’Mau a Mulungu ? ( Ŵelengani 1 Timoteyo 5 : 23 . ) Tsopano tiyeni tikambilane mmene kucita zinthu ziŵilizi kumalimbitsila ubwenzi wathu ndi Yehova . Tikakumana ndi ciyeso , tingazindikile kuti tifunika kukhala oleza mtima kwambili , oyamikila , kapena acikondi . Mgwilizano wa Zipembedzo , 3 / 1 M’nkhani ino , tikambilana mfundo zotsatilazi : mmene tingalimbitsile cikhulupililo cathu , mmene tingaonetsele kuti cikhulupililo cathu n’colimba , ndiponso mmene tingakhalile otsimikiza mtima kuti Mulungu adzayankha tikam’pempha kuti ationjezele cikhulupililo . Pamene mucita ulaliki umenewu , nthawi zambili anthu amakhala omasuka kudzatenga mabuku athu ngati mumwetulila na kuwapatsa moni mwaubwenzi . Njila yoyamba imene tingalimbitsile mgwilizano wa anthu a Mulungu ni kukhala odzicepetsa . Aonetseni kuti ndi ofunika kwa inu . Kodi Aisiraeli okhulupilika anaonetsa bwanji kuti anakanilatu kucita zosalungama ? ( Onani bokosi yakuti “ Mmene Mungakulitsile Luso Loimba . ” ) ( b ) Ni mfundo ziti zimene muona kuti zingakuthandizeni ngati mau anu samveka bwino ? Tikutelo cifukwa cakuti palibe colakwika ciliconse ndi mmene pulaneti lathu linalengedwela . “ Ici cidzacitika ngati mudzamvela mwacangu mau a Yehova [ Mulungu ] wanu . ” — ZEK . Posapita nthawi , makolo athu anazindikila kuti iye amayendetsa maso ake mofulumila kwambili pofuna kuwauza zimene akuganiza ndi mmene akumvela . Cikondi sicicita nsanje , sicidzitama , sicidzikuza , sicicita zosayenela , sicisamala zofuna zake zokha . ” ( b ) Kodi tiphunzilapo ciani tikaganizila mmene Yehova anapulumutsila Hezekiya ndi anthu ake ? Azilongosi ake anali kum’teteza kuti asagwe m’ciyeso ndi kucita chimo . ( 1 Akor . 16 : 2 ) Mwezi uliwonse mipingo imatumiza zopeleka zimenezi ku ofesi ya Mboni za Yehova m’dziko lao . ( Yoh . 6 : 44 ) Ngati muceleza munthu cifukwa comukonda , ubwenzi wanu na iye umalimba . 6 : 8 - 15 ; 7 : 54 - 60 . Conco , Khoti Yapamwamba ya Ayuda inapatsidwa ulamulilo waukulu . Mwacitsanzo , Baibulo limati “ kucita maseŵela olimbitsa thupi n’kopindulitsa pang’ono . ” Komabe , mfundo zimene tafotokoza zikhudzanso aja amene amatafuna kapena kufwenkha fodya amene ali ndi nikotini . [ Mau okopa papeji 4 ] ( Yona 1 : 17 – 2 : 10 ) Mungaŵelengenso pemphelo locokela pansi pa mtima limene Solomo anapeleka kwa Yehova popeleka kacisi . ( 1 Maf . Mfundo yakuti Yehova amatsogolela nchito yathu , sitanthauza kuti iye nthawi zonse amasintha zocitika za m’dziko kuti atithandize kulalikila . Nthawi zambili , a Mboni za Yehova amaona maumboni oonetsa kuti angelo amawathandiza pa nchito yawo yolalikila . Cifukwa cosadziŵa bwino cinenelo , Osei sanapeze nchito yabwino kwa caka cimodzi . Caposacedwa , abale na alongo masauzande ambili , kuphatikizapo ana , anathaŵa nkhondo ndi cizunzo m’cigawo ca kum’mawa kwa dziko la Ukraine . Timoteyo anakhala ndi mbili yabwino cifukwa cogwila nchito mwakhama , kudzicepetsa , ndi kupilila mokhulupilika panthawi zovuta . Mosiyana ndi anamwali opusa , anamwali asanu anali okonzekadi cifukwa anali ndi mafuta ena m’mabotolo ao kuonjezela pa mafuta amene anali kale m’nyali zao . M’malomwake , iwo amatengela citsanzo ca Yehova . Smong ! ” 4 : 6 ) Ngati ticita zimenezi , ndiye kuti tikuikabe maso athu pa Yehova . Koma anthu ena anadziŵa kuti moyo ndiwo unali wofunika kwambili cakuti anacita zomwe angathe kuti apulumutse anthu . M’malo mokaniza cikhumbo coipa cimeneco , Akani anaba katunduwo cifukwa ca umbombo ndi kukaubisa m’hema wake . Komabe , nthawi zina tingaone zinthu molakwika n’kumaganiza kuti munthu wina mumpingo kapena ise , tacitilidwa zinthu zopanda cilungamo . 10 : 29 . Kodi makolo angatsatile motani citsanzo ca Yehova , M’busa Wamkulu ? Anam’patsa ndi “ Wamasiku Ambili , ” Yehova Mulungu . * ( Danieli 7 : 13 , 14 ) . Anafunika kuthaŵila ku mzinda wothaŵilako wapafupi na kwawo . Kucokela panthawiyo , ndinayamba kukumana ndi mavuto monga kuona zideludelu , mutu kuŵaŵa , kumva kupweteka m’thupi , ndi mavuto ena obwela cifukwa coleka kukoka ndi kumwa moŵa . 1 , 2 . ( a ) Kodi mabanja ambili amakumana ndi mavuto otani ? Ndipo pangabuke funso liti ? 10 : 23 ) Conco , ndi bwino nthawi zonse kupemphela , kutsatila citsogozo ca mzimu woyela , ndi kumvela mau a Yehova . Zinthu zonse zinali ngati kuti anapangila anthu aatali kuwilikiza kaŵili pa msinkhu wanga . Onse anali kufuna kuti tipite ngakhale kuti zikanativuta kuwasamalila tili kutali . Popeza Akhiristuwo anali akali na moyo padziko lapansi , kodi anali “ ngati akufa ku ucimo ” m’lingalilo liti ? Monga takambila m’nkhani ino , timapitiliza kugwila nchito yolalikila kuti tilemekeze Yehova na kuyeletsa dzina lake , komanso pofuna kuonetsa kuti timakonda Yehova na Yesu . Cinanso , timalalikila pofuna kucenjeza anthu na kuonetsa kuti timawakonda . Cifukwa ku mbali yathu kuli magulu ankhondo okwela pa mahosi . 14 : 1 , 18 . N’cifukwa ciani citsanzo ca makolo n’cofunika ngako pophunzitsa mwana ? Yoshiko anali kukhala pa mtunda wa makilomita pafupifupi 40 kucokela pa Nyumba ya Ufumu , ndipo nyumba yake inaonongeka . 25 : 8 ; 33 : 24 ) Ganizilani mmene tidzasangalalila pamene Yehova adzaononga adani ake onse ndi kutiloŵetsa m’dziko latsopano la mtendele ndi la cilungamo . Cipembedzo conama cimaipitsa dzina la Mulungu ndi kupotoza zimene Mau ake amakamba . 24 : 14 ) Paulo anatetezanso uthenga wabwino ndi kulengeza za cikhulupililo cake kwa bwanamkubwa Porikiyo Fesito , ndi pamaso pa Mfumu Herode Agiripa . Inoki anakamba ulosi umenewu monga kuti wacitika kale cifukwa zimene anali kukamba zinali zakuti zidzacitikadi zivute zitani . — Yesaya 46 : 10 22 : 3 . ( When Egypt Ruled the East ) Kuti Aiguputo azimuopa Farao , iye anali kuvala cisoti cacifumu cokhala ndi cifanizo ca njoka imene ifuna kuluma munthu . Conco , makolo muzithandiza ana anu kuonetsa kuwala kwawo mwa kuwaphunzitsa kupeleka ndemanga m’mau awo - awo . Kodi pemphelo liyenela kukhala cizolowezi cabe kapena kukhala ngati mankhwala amene angatithandize kumvelako bwino tikadwala ? Tiphunzilapo ciani pa nkhani ya Mfumu Davide ? Ndili kumeneko , mnzanga wina amene anali kugwilila nchito kophikila makeke , dzina lake Rudolf Tschiggerl , anayamba kuceza nane nkhani za m’Baibulo . Knorr anakambako zokhudza mlandu umene abale anapambana mu Khoti Lalikulu kwambili ku United States . Kodi adziŵa mapindu amene angapeze , komanso mavuto amene angakumane nawo cifukwa cokhala Mkhristu ? Mwadziŵa kuti khalidwe lake lalikulu ndi cikondi , ndi kuti anakupatsani Mwana wake kuti akhale dipo lanu . Kudzela m’magazi a Yesu , Yehova anandikhululukila . Koma udzaphwanya ndi kuthetsa maufumu ena onsewo [ a anthu ] , ndipo udzakhalapo mpaka kalekale . ” kapena , ‘ N’cifukwa ciani siticitako zinthu zina zimene anthu ena amacita , monga kuvota , kuti tikonze zinthu padzikoli ? ’ Kodi anthu osalakwa amenewa ali ndi ciyembekezo cotani ? ( Ŵelengani Machitidwe 24 : 15 ) Nanga n’cifukwa ciani adzaukitsa akufa ? Popeza iye ndi wangwilo sanafunikile kukhululukidwa macimo . Kodi anthu amene amaseŵenzetsa ufulu wawo mwanzelu ali na tsogolo lotani ? Ambuye wathu anati : “ Munthu sangakhale ndi moyo ndi cakudya cokha , koma ndi mau onse otuluka pakamwa pa Yehova . ” ( Mat . N’cifukwa ciani tiyenela kukhalabe maso ngakhale tione kuti tayembekezela kwa nthawi yaitali ? Pamene Yesu anali kulalikila pa Phili , anaphunzitsa ophunzila ake kuti ayenela kukhala mwamtendele ndi kupewa mikangano ngakhale ataona kuti zinthu sizingawayendele bwino akacita zimenezo . Kelsey anapeza thandizo pa Miyambo 13 : 16 , imene imati : “ Aliyense wocenjela amacita zinthu mozindikila , koma wopusa amafalitsa ucitsilu . ” 10 : 7 ) Ataukitsidwa , Yesu ananenelatu kuti otsatila ake adzalengeza uthenga umenewu “ mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ” ( Mac . Rutherford ndi W . Iye anati : “ Zakhala zolimbitsa cikhulupililo kwambili kuona mmene Yehova akutithandizila pa umoyo wathu . ” Nayenso Timoteyo anali munthu wophunzitsika , n’cifukwa cake Paulo anam’konda . Analeka kuganizila kwambili zinthu zimene zinali kumucititsa kuti aziopa . Tsiku lina poyenda m’mbali mwa nyanja , n’nakumana ndi Mboni za Yehova zambili za m’makampu ena . ( b ) N’cifukwa ciani Mulungu anapangila Adamu mkazi ? 50,500,000 Musaiŵale kuti Abulahamu anaika maganizo ake pa “ mzinda wokhala ndi maziko enieni . ” Anthu ena akambanso zofanana ndi mfundo imeneyi . Ponena za ciweluzo cimene cidzacitika mkati mwa cisautso cacikulu , Yesu anakamba kuti anthu “ adzaona Mwana wa munthu akubwela pamitambo ya kumwamba . ” Pamene anayamba kucita zimenezo mu 1993 , mumzinda wa New York munali kagulu ka ofalitsa 20 cabe okamba Cirasha . Cifukwa ca zimenezi , Yunike ndi Loisi pamodzi ndi Timoteyo anakhala Akristu . Ngakhale kuti anthu opita ku maiko ena zimawapweteka mtima kusiya mnzao wa m’cikwati kapena ana , io amaona kuti amafunikabe kupita . Mulungu Amakudziŵani 5 Anakambanso kuti : “ Magazi ake anali kukhala pamutu pake , cifukwa sanagwilitsile nchito makonzedwe a Mulungu omuteteza . ” Tifunikanso kukhala osamala ndi zimene timakamba ndiponso mmene timakambila ndi ena . 4 : 4 ) Tiyenela kuphunzila mmene tingatsatilile mfundo za m’Baibulo paumoyo wathu . 15 : 31 ) Pocita zimenezi , Yesu sanali kucotsa ciwalo coonongeka ndi kuikapo cina . Mboni ina yokangalika ya zaka 84 ya ku Norway dzina lake Kåre inati : “ Ndimaona kuti ndi mwai waukulu kutumikila Yehova , Mfumu yacilengedwe conse , ndi kukhala pakati pa anthu odziŵika ndi dzina lake loyela . M’bale Mumba : Inde . Baibulo limatiuza kuti iye “ amatitonthoza m’masautso athu onse . ” M’kupita kwa nthawi , ena mwa anthu amenewo anakhala Mboni . Tinasangalala kwambili polela ana athu ndipo tinali kuyesetsa kucitila zinthu pamodzi nthawi zonse . Insight on the Scriptures — Buku limeneli lili na zigawo ziŵili , ndipo limafotokoza za anthu , malo , na mau opezeka m’Baibo Ndiyeno anati : “ Kuyambila ku Yerusalemu Inu mudzakhala mboni za zimenezi . ” — Luka 24 : 44 - 48 . Makolo ena ku South Africa , polima m’dimba ndi atsikana awo aŵili , amawafotokozela kudabwitsa kwa mbewu , mmene zimamelela ndi kukula . Anthu ena okonda cilungamo nawonso akhumudwa ndipo sakumvetsa cifukwa cake munthu wosalakwayo ndi ana ake akuphedwa . Mtundu wa anthu unakhalanso na ciyembekezo . Izi zinandithandiza kuyamba kuona zinthu moyenela ndi kumvetsa kuti makolowo anali kunditsutsa cifukwa condidela nkhawa . Yesu anakamba mosapita m’mbali pa malamulo onse a anthu amenewo . Ngakhale Akhristu oona masiku ano , cikondi cawo cikhoza kuzilala monga mmene zinalili kwa Akhristu oyambilila a ku mpingo wa Efeso . Iye anakambanso kuti : “ Ndipo zina zonsezi zidzaonjezedwa kwa inu . ” 21 Limbitsani Cikhulupililo Canu pa Zimene Muyembekezela ( Sal . 32 : 2 ) Inde , anthu amene amacotsa cinyengo ciliconse m’mitima yao amakhala acimwemwe , ndipo adzakhalanso ndi cimwemwe ceniceni mtsogolo . Tikamaonetsa cikondi kwa anzathu , timaonetsa ulemelelo wa Mulungu . Mika anadziŵa kuti pa iye yekha sakanakwanitsa kuthetsa makhalidwe oipawo . NYIMBO : 133 , 43 Ngakhale n’conco , cizunzo sicinaletse kufalikila kwa coonadi . Ambili angatilimbikitse kukhala na colinga copeza nchito yapamwamba , imene ingaticititse kukhala na mphamvu zolamulila ena , kukhala wochuka , ndi wolemela . Iye wakhala akutsogolelanso nchito yolalikila uthenga wa Ufumu m’maiko okwana 239 ndipo waphunzitsanso anthu mamiliyoni ambili ponena za njila za Yehova . Komabe , abale na alongo athu amayamikila ngati tipewa kuvala zovala zothina , zotayilila kapena zoonetsa thupi . Pakuti ngakhale kuti masautso amene tikukumana nao ndi akanthawi ndipo ndi opepuka , masautsowo akuticititsa kuti tilandile ulemelelo umene ukukulilakulila komanso wamuyaya . ” — 2 Akor . Posacedwapa atumiki a Yehova adzagwila nchito yopindulitsa kwambili tsiku lililonse . Mbili ya makono ya Mboni za Yehova , ionetsa kuti ocepa acotsedwa mu mpingo cifukwa cosatsatila miyezo ya Mulungu . Ndikuona kumwamba kotseguka , ndipo Mwana wa munthu waimilila kudzanja lamanja la Mulungu . ’ ” — Machitidwe 7 : 55 , 56 . 14 : 2 , 11 ) Zoonadi , Yehova ndiye anasankha Mose , Yoswa , Gidiyoni , ndi Davide kuti amuimile monga Mtsogoleli . Mosiyana na zimenezi , wamasalimo anati : “ Wodala [ wosangalala ] ndi munthu amene thandizo lake limacokela kwa Mulungu wa Yakobo , amene ciyembekezo cake cili mwa Yehova Mulungu wake . ” — Sal . Afunika kuphunzitsidwa kulalikila uthenga wabwino , ndi mmene angaphunzitsile ena coonadi . Kuyambila kale - kale , anthu a Mulungu akhala akucilikiza ucifumu wake . Polembela Akristu anzake , iye anati : “ Nthawi zonse tikamakupemphelelani timayamika Mulungu , Atate wa Ambuye wathu Yesu Kristu . ” ( Yes . 43 : 10 ) Khalidwe la mwana lingapangitse kuti anthu azilemekeza makolo ake kapena kuwanyoza . Mukamafotokoza maganizo anu , muzisankha bwino mau kuti akhale “ okoma ngati kuti mwawathila mcele . ” Mwacitsanzo , mpingo wina uli na ofalitsa 134 , koma gawo lawo lili cabe na nyumba 50 . Mungathandize Ena Mumpingo Wanu , Mar . Anthu ena adzaona makhalidwe anu abwino , ndipo ambili adzalemekeza Atate wathu wakumwamba . — Mat . Mwina mungadzifunse kuti , ‘ Kodi mfundo za m’Baibo zingakhale zothandiza masiku ano ? ’ Yesu nayenso anali kusalidwa ndi anthu ena . Kuwonjezela pa nchito yomanga kacisi , Aisiraeli anafunikanso kumanga mizinda yawo . Makolo , kodi mungawathandize bwanji ana anu kukonzekela ubatizo ? Mlongo wina wa ku Brazil , dzina lake Rachel , anati : “ N’nali kukonda kwambili mafashoni a kudziko , ndipo sin’nali kuvala mwaulemu . Mtsikana wina dzina lake Jessica anati : “ Atate na amayi amakondana na kulemekezana maningi . Nanga zinthu zimuyendela bwanji Choong Keon ndi mkazi wake Julie , amene tachula kuciyambi kwa nkhani ino ? Kuŵelengela munthu lemba losankhidwa bwino kumakhala kothandiza ngako kuposa ciliconse cimene tingakambe . Timaonetsa kuti ndife odzipeleka kwa Mulungu mwa kulambila iye yekha cabe . ( b ) Kodi citsanzo ca mtumwi Petulo na malangizo amene anapeleka zingatithandize bwanji ? Comfort anati : “ Ayuda anali kukonda kuika mipukutu ya Malemba m’mitsuko kuti isungike bwino . ” Patapita miyezi yocepa , anasamukila ku Massachusetts kukatumikila kumpingo umene unali na ofalitsa Ufumu ocepa . Ngakhale kuti Yesu anali kudziŵa kuti ambili mwa iwo sadzalabadila uthenga wake , iye anapitilizabe “ kuwaphunzitsa zinthu zambili . ” — Maliko 4 : 1 - 9 . Tikakumana ndi mavuto aakulu , tidzakhalabe na cimwemwe ngati tiganizila zimene Yehova waticitila komanso kumuyamikila . N’kulakwa kuganiza kuti sitingakwanitse kulimbikitsa ena cifukwa cakuti ndise osamasuka kweni - kweni na ŵanthu . Kucoka mu 1952 kufika mu 1956 , Maria anali kugwila nchito yakalavula gaga m’ndende ya pafupi na mzinda wa Gorkiy , ( umene lomba umachedwa kuti Nizhniy Novgorod ) ku Russia . Mofananamo , Yehova ndiye cikondi , koma “ amalanga aliyense amene iye amamukonda . ” N’cifukwa ciani tingakhale otsimikiza kuti Paradaiso imene tiyembekezela padziko lapansi si maloto koma ni yeni - yeni ? Abale ndi alongo ambili ayamba upainiya wa nthawi zonse kapena wothandiza . 5 : 19 - 21 ) M’kalata yoyamba imene Paulo analembela mpingo wa ku Korinto , iye anafotokoza makhalidwe ena amene anthu akuthupi amakhala nawo . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Anthu okhwima mwauzimu . . . amene pogwilitsa nchito mphamvu zawo za kuzindikila , aphunzitsa mphamvuzo kusiyanitsa coyenela ndi cosayenela . ” — Aheberi 5 : 14 . Anna anati : “ Titaona khama la atate lofuna kukhala kholo labwino ndi kulimbitsa cikondi m’banja , tinayamba kuŵaona moyenela . Mwana wawo anayamikila ngako . Masiku ano , akucita umishonale ku Mozambique . N’cifukwa ciani anali kutsutsa zakuti iye analikodi ? ( 2 Mbiri 11 : 21 - 23 ) Pamenepa , Rehobowamu anacita zinthu mozindikila kusiyana na mmene anacitila m’mbuyomo . Conco , pambuyo pomvetsetsa nkhani yonse , akulu anali kuganizilanso za munthuyo , osati za colakwa cake cabe . ( Gen . 41 : 51 , 52 ) Cifukwa cakuti Yosefe anakhalabe wokhulupilika kwa Mulungu , anadalitsidwa kwambili . Cifukwa ca madalitsowo , iye anapulumutsa Aisiraeli ndi Aiguputo . Zinthu zimenezi ziphatikapo ziphunzitso zabodza , nzelu za anthu , makhalidwe oipa monga ciwelewele , kupepa fwaka , kukolewa , ndi mankhwala osokoneza ubongo . Mabanja acikhiristu ayenela kupewelatu mzimu wa dziko . ( Aef . Yesu wasankha akulu kuti azitsogolela mpingo , ndipo amafuna kuti tiziwalemekeza ndi kutsatila malangizo amene amatipatsa . Moyenelela Yesu anawacha kuti onyenga cifukwa sanali kufuna kumva yankho la funso lao , koma anali kufuna kuti “ am’kole m’mawu ake . ” — Mateyu 22 : 15 - 22 . Jonathan anakamba kuti , “ Pamene Bizinesi yathu inatha , n’nali na nkhawa kwambili . N’cifukwa ciani Yehova amalola kuti tizilimbana ndi zofooka ? N’ciani cingatithandize kuona Yehova ndi dzanja lake ? Yesu anauza atumwi ake okhulupilika kuti : “ Ndikupita kukakukonzelani malo . Onani kuti Yesu poyankha anayamba ndi kufotokoza za makolo akale amenewo ndi mau akuti , “ kunena za kuuka kwa akufa . ” 5 : 33 - 37 ; 23 : 16 - 22 . Ofalitsa ena , zimawavuta kupeza munthu woti amulalikile akakhala mu ulaliki wa khomo ndi khomo . Kodi anafuna kuti aliyense azilalikila payekhapayekha kapena monga gulu logwilizana ? Koma mwana wao woyamba atabadwa , io analeka kucita upainiya ndipo tsopano ali ndi mwana waciŵili . Simunandipatse mbeu . ” M’dziko latsopano , aliyense azikagaŵana zinthu na anzake . 11 : 29 , 30 ) Aliyense wofuna kulambila Mulungu m’njila yoyenela afunika kuzindikila na kuvomeleza udindo wa Yesu pokwanilitsa colinga ca Yehova . Kuphunzila Malemba sikutithandiza cabe kudziŵa mbali imene tiyenela kuongolela . “ Imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . ” — Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . Sikuti zonse zochulidwa pamenepa zimaonekela mwa wodwala aliyense kapena mmene azindandalikila iyai . 11 : 3 . Cifukwa cakuti abale anali kulalikila mwakhama , coonadi cinayamba kupita patsogolo . Timayamikila Yehova cifukwa cotithandiza kukhalabe okhulupilika panthawi yovuta kwambili imeneyo . Eduardo sanafune kuyamba nchito imene ikanam’cititsa kukhala kutali ndi banja lake kwa miyezi kapena zaka zambili . Ndipo pa tsiku la nkhani , ndeke ziŵili zinamwaza tumapepala toitanila anthu m’dela lonse tokwanila 100,000 . Nkhanizi ndi njila imodzi imene Yehova amatithandizila kuti tikwanilitse nchito yaikulu imene watipatsa . ( Sal . Kukonda Yehova kudzatithandiza kuti tizipemphela kwa iye nthawi zonse . Mofanana ndi kanjele ka mpilu kamene “ ndi kakang’ono kwambili mwa njele zonse , ” mpingo wacikristu unali waung’ono kwambili pamene unayamba mu 33 C.E . Komabe , iye anali kufunika kufotokozela akulu nkhaniyo . Zimenezo zinandithandiza kuti ndimvetsele ndi kugwilitsila nchito malangizo a m’Baibulo amene anandipatsa . ” ▪ Kodi Mumakhulupilila Kuti Muli ndi Coonadi ? Pocititsa kulambila kwa pabanja , kholo lifunika kumbukilani kuti malangizo amene mwana angafunikile amasiyana na amene wacinyamata amafunikila . ( Miy . 15 : 3 ) Ndiye cifukwa cake Paulo sanadodome kulembela Akorinto kalata yoyamba . Ndiyeno analata kutsidya la cigwa , n’kukamba kuti : ‘ Apo , cakumanzele kwathu , ndiye pali mabwinja a Soko . ’ Kodi makhalidwe a cipatso ca mzimu woyela angakuthandizeni bwanji kulimbana kapena kupewa zinthu zobweletsa nkhawa ? Anapeleka malangizo amenewa pa ulaliki wake wa pa Phiri . David : Nchito imene tinali kugwila pa famu yathu kwa zaka zonsezo inali yovuta , koma tinayesetsa kukhala citsanzo cabwino kwa atsikana athu pankhani yolambila Yehova . YOSIMBIDWA NDI Christof Bauer Ndithu ndikuthandiza . ” Akapeleka moni ndi kudzidziŵikitsa , iye amapatsa mwininyumba kapepala kauthenga kakuti , Kodi Mufuna Kudziŵa Mayankho Azoona pa Mafunso Aya ? Wamasalimo anati : “ Wodala ndi munthu amene Yehova sanamusungile colakwa cake , amene alibe mtima wacinyengo . ” Nkhani yoyamba pa nkhani ziŵilizi idzafotokoza fanizo la Yesu la mpesa ndi la wofesa mbeu , ndipo idzalongosola mfundo zimene tiphunzilapo zokhudza nchito yathu yolalikila . Izi zinatithandiza ngako . ” Koma mwina mwamvapo ena akukamba kuti , “ Adzaona cimene cinameta nkhanga mpala . ” Ndipo anali kusilila mwa nsanje komanso kucita macimo . — Aroma 1 : 28 , 29 . Ife sitinali oyenelela kuonetsedwa cikondi cimeneco , komanso sitingakwanitse kumulipila . 10 : 16 ; 2 Akor . 5 : 15 ; Mat . ( Aheb . 10 : 24 ) Conco , tifunika kudziŵa bwino macuni na mau a m’nyimbo zathu . Koma anali kukonda kwambili zosangulutsa cakuti analeka kugwilizana ndi anthu a Yehova . ( Deuteronomo 7 : 1 - 4 ) Aisiraeli ambili anayamba kutengela zocita za Akanani amene anali kulambila mafano ndi kucita zinthu zina zoipa . — Ŵelengani Salimo 106 : 34 - 39 . Iye anali kuganizila za anthu a ku Filipi . 20 : 7 , 8 . Koma bwanji ngati takhala tikupempha thandizo pa vuto limene lativuta kwa nthawi yaitali ? Koma lomba , Adolfo amalimbikitsa ena kukhala ofatsa mwa mau na citsanzo cake cabwino . Magazini a Galamukani ! Tiyeni tikule m’zinthu zonse , kudzela m’cikondi , pansi pa iye amene ndi mutu , Khiristu . ” ( Ŵelengani Malaki 3 : 16 . ) M’malomwake , iye anagwilitsila nchito njila zosiyanasiyana kuti am’thandize kuyamba kuphunzila Baibulo . Zoonadi , Mulungu amatitonthoza tikapemphela kwa iye . Ndipo anatiuza kuti tiyenela ‘ kumva zimene mzimu ukunena ku mipingo . ’ Koma ndi cikondi cotani cimene ayenela kusonyezana ? Sitimakamba cabe kuti ndife ogwilizana koma timasangalaladi ndi mgwilizano weni - weni pakati pathu . M’nkhani yotsatila , tidzaphunzila mmene cikhulupililo cingatithandizile kuliona bwinobwino dzanja la Yehova pa umoyo wathu . Kirsten anapempha thandizo kwa ena mu mpingo , amene nawonso amatumikila Yehova . Ponena za nthawi imene odzozedwa onse adzakhala kumwamba , lemba la Chivumbulutso 17 : 14 limanena zimene zidzacitikila adani a anthu a Mulungu . N’zoona kuti anthu anali kumvetsela Baibo ikuŵelengedwa akapita ku chechi . Zotsatilapo zake ndi zakuti , ndili pa ubwenzi wabwino ndi anthu ambili . Coyamba , imatipatsa malangizo amene angatithandize pa umoyo wathu wa tsiku na tsiku , ndipo caciŵili , imatithandiza kudziŵa Mulungu ndi malonjezo ake . — 1 Timoteyo 4 : 8 ; Yakobo 4 : 8 . Anthu atalengedwa , mngelo wina anayamba kulaka - laka kuti anthu azimulambila . Conco , iye anapandukila Yehova n’kukhala Satana , kutanthauza kuti “ Wotsutsa . ” Ahabu anaona zimenezo . Kumbukilani kuti kuimba nyimbo ni mbali yofunika pa kulambila kwathu . Tsopano kwa nthawi yoyamba , Yehova anaonetsa mbali imene Sara anali nayo . Ngakhale n’nali kukhulupilila zimene Amayi anali kutiphunzitsa , sin’nali kuziona kuti n’zofunika . Conco , Eliya anauza Ahabu kuti Mulungu wanena kuti ‘ adzaseselatu ’ kapena kuonongelatu anthu onse a m’banja la Ahabu . 19 : 32 - 35 ) Abulahamu anataikilidwa mkazi wake ndipo Naomi anafedwa mwamuna wake . — Gen . Koma ambili a iwo sakhala okondwela na nchito yawo . Ndipo Baraki anatsikadi m’phili la Tabori , amuna 10,000 akum’tsatila . ” — Oweruza 4 : 14 . ( Aheb . 10 : 24 , 25 ) Panali patatsala zaka 5 cabe kuti Akhristu aciyuda okhala mu Yerusalemu aone cizindikilo cimene Yesu anawapatsa coonetsa kuti “ tsiku . . , la Yehova ” layandikila , ndipo anafunika kuthaŵa mu mzindawo kuti apulumutse miyoyo yawo . ( Mac . Conco tingafunse kuti , N’zinthu ziti zimene zingabweletse “ nsautso m’thupi , ” imene Paulo anakamba ? Akaziwa anamvela Mulungu m’malo momvela Farao ndipo anapulumutsa anawo . Nanga Mboni zakwanitsa bwanji kutsatila miyezo ya pamwamba imeneyi ? 51 : 12 , 13 . Nafenso timapindula ndipo timaphunzilanso zambili kwa abale a kumeneko . ” Ndinayamba kufufuza colinga ca moyo , ndipo zimenezo zinandipangitsa kulephela kukhazikika pamalo amodzi . Iye amatithandiza olo pamene takumana na mavuto aakulu kwambili . — Sal . Koma amadelanso nkhawa za thanzi la mayi na mwana wodzabadwayo . Komabe , anali kukaikila ngati angakwanitse kucita zimenezi . Iye , amene ni wacifundo kwambili kuposa aliyense , anauza anthu ake kuti : “ Ineyo ndi amene ndikukutonthozani anthu inu . ” — Yes . ( Yobu 2 : 7 ) Ngakhale kuti Yobu analakalaka kufa , anali ndi cikhulupililo cakuti Mulungu adzamuukitsa n’kukhalanso ndi moyo . Mavuto a moyo uno amacititsa anthu ambili kusoŵa mtendele Komabe , mosasamala kanthu za kumene mumakhala , ngati mumapatula nthawi yoceza ndi wophunzila ngakhale kuti mumakhala ndi zocita zambili , iye adzadziŵa kuti mumamuona kukhala wofunika . Naye mlongo Margaret anakamba kuti : “ Muziceza ndi amishonale kapena apainiya amene ni aciyambakale . ‘ Iwo anaona kuti ngati gulu la Yehova lapanga masinthidwe , ndi bwino kuvomela mosavuta m’malo motsutsa . ’ ” Akhristu sacotsa mimba cifukwa kutelo n’kuononga moyo wa mwana wosabadwa . ( Eks . ( Aroma 6 : 23 ) Nthawi ina , zimenezi zinapangitsa mtumwi Paulo kuvutika kwambili maganizo . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kudzicepetsa ? Makolo ake , abale ndi alongo ake onse anali opanda ungwilo . Kuleka khalidwe limeneli kwam’thandizanso kupewa ciwelewele . 15 , 16 . ( a ) Kodi anthu ena adzacita ciani akaona kuti ndife okhulupilika kwa Mulungu ? Komabe , ana amene amasamalila makolo ao sayenela kunyalanyaza udindo wosamalila mabanja ao . Koma ngati sitiyamikila zimene io amacita , cikhumbo cao cokalamila mautumiki ena , monga mmene Baibulo limawalimbikitsila , cimacepa . — 1 Tim . Kodi cikondi cimene timaonetsa kwa ena cingawathandize bwanji kuphunzila za Yehova ? ( b ) Mofanana ndi mwana wa Yefita , n’ndani masiku ano amene ayenela kulimbikitsiwa ? CIKUTO : Alongo alalikila m’Cirasha , m’mbali mwa nyanja ku Tel - Aviv . 9 , 10 ) Umu ni mmene zinthu zinalili pamene Yohane analembela Gayo kalata . 8 : 12 , 13 ) Inde , ngati tikhalabe odzicepetsa , ife pamodzi ndi anthu ena okhudzidwa na nkhaniyo , tidzapindula kwambili . — Ŵelengani 1 Petulo 5 : 5 . Mwacitsanzo , mukuthandiza oukitsidwa kudziŵa Yehova . ( Yoh . 17 : 3 ; Mac . AKATSWILI OFUFUZA amalosela mmene malonda ndi ndale zidzayendela . Patapita nthawi , anafunsila kuti akathandize pa nchito yomanga malo olambilila m’maiko ena koma sanaitanidwe . Ngakhale pamene mfumu inamusankha kukhala mfumukazi yake , iye sanadzitukumule kapena kunyadila ena ayi . — Esitere 2 : 9 , 12 , 15 , 17 . Kumbukilani zitsanzo zitatu za anthu amene tawachula poyamba aja . “ Ndinaona anthu akuonetsana cikondi ceniceni . ” ​ — PANAYIOTA Anatinso : “ Pakuti ngakhale Khiristu sanadzikondweletse yekha . ” Iwo ananilandila na manja aŵili . Iye ndiye kasupe wa moyo wathu . Popanda iye sitikanakhalako . ( Mac . Malo na Nyumba : Mungapeleke ku gulu la Mboni za Yehova malo na nyumba zimene angagulitse . Kenako , anatsekapo na civininkhilo colema cija camtovu . Muthandizeni kudziŵa kuti ndi wofunika kwambili mumpingo . N’nakondwela kutumikila na m’baleyu , amenenso analandila fomu yanga yofunsila utumiki wa pa Beteli pa msonkhano wa cigawo mu 1955 . Nkhuku ikaona kamtande akuuluka m’mwamba imalila mokweza kucenjeza ana ake , ndipo anawo amabwela mwamsanga kukabisala m’mapiko ake . 106 : 9 - 11 ) Zimene zinacitikazo zinali zodabwitsa kwambili cakuti ngakhale pambuyo pa zaka 40 , anthu anali kukambabe za cocitikaco . 38 : 8 - 12 , 16 . Iwo amaona kuti ni mwai kucha Yehova kuti Atate wawo , ndipo afuna kuti iye aziwaumba . Kodi n’natsatila mfundo za dziko kapena za Mulungu ? ’ — Agal . 4 : 7 ) Cikondi cimeneci ndiye capamwamba kwambili . Ni mmenenso amacitila masiku ano . Alongo ambili amene anatumikilapo ku dziko lina , poyamba anacita mantha kupita ku dziko lacilendo . Zimene Baibo imakamba Yesu atatsala pang’ono kuphedwa , iye anaima na kuyang’ana Yerusalemu , mzinda waukulu wa Ayuda . ( Yobu 35 : 7 ) Kodi pamenepa Elihu anali kutanthauza kuti zimene timacita potumikila Mulungu n’zopanda phindu ? Kodi imapambana mphatso zina za Mulungu m’njila yabwanji ? Amazindikila kuti sangakondweletse Yehova ngati iye ndi kapolo wa zizoloŵezi zoipa . Kodi ndi cikondi ca pakati pa mabwenzi apamtima ? ( Yoh . Mwacitsanzo , Richard akukumbukila zimene anakambilana ndi Mboni za Yehova ziŵili . Buku ina yaposacedwa yokamba pa cipembedzo ku America inati : “ Atsogoleli acikhiristu akhala akusintha ziphunzitso zawo kuti zigwilizane ndi zikhulupililo ndi maganizo a mamemba awo ndi anthu ambili . Amacita izi kuti iwo awacilikize . ” Onani mmene Baibulo limafotokozela cimene cingasonkhezele wina kucita zoipa , pamene limati : “ Munthu aliyense amayesedwa mwa kukopedwa ndi kukodwa m’cilakolako cake . Ni zifukwa ziti zimene inu muli nazo zofuulila kuti “ Tamandani Ya ” ? “ Walimbana ndi Mulungu ndi anthu , ndipo potsilizila pake wapambana . ” — GEN . Munthu wina amene anaika maganizo ake pa zinthu zakumwamba ndi Mose . Mkulu wa apolisi anati : “ Ane mpunga uwu popeza wamangidwa cifukwa ca Mau a Mulungu . N’zocititsa cidwi kuti Malaki anakamba kuti Yehova ‘ amachela khutu ndi kumvetsela ’ pamene anthu ake akukambilana wina na mnzake . ( Mal . ( b ) N’cifukwa ciani Yehova sadalila amtolankhani a dziko ? Kodi mukali ndi maganizo otelo ? Sikuti iye ali cabe mulungu wamphamvu kuposa milungu ina . Iye anati : “ Khalani ndi khalidwe labwino pakati pa anthu a m’dzikoli , kuti . . . pokhala mboni zimene zikuona ndi maso zocita zanu zabwino , adzatamande Mulungu . ” ( 1 Pet . Kwa zaka 100 zapitazo , anthu oposa 100 miliyoni anaphedwa pankhondo . Susan amacita mantha kuyenda pa ndeke , koma timayenda pa ndeke kaŵilikaŵili . Tingatengelenso cikhulupililo ca Mariya mwa kumvetsela mosamala kwambili kwa Yehova , ndi kusinkhasinkha zinthu zimene taphunzila zokhuza iye ndi zolinga zake . Baibulo imapeleka malangizo aya : “ Mkazi asasiye mwamuna wake , koma ngati angamusiye , akhale conco wosakwatiwa . Apo ayi , abwelelane ndi mwamuna wakeyo . Mwamunanso asasiye mkazi wake . ” ( 1 Akor . [ 2 ] ( ndime 11 ) Kuti mudziŵe zambili pankhani ya kubadwanso , onani Nsanja ya Olonda ya April 1 , 2009 , tsamba 3 mpaka 11 . Woyang’anila dela wina anati : “ Masiku ano , anthu ambili m’dela lathu amafunitsitsa kuti zinthu zisinthe pa zandale . Ojambula zithunziwo sanali kudziŵa mmene Yesu anali kuonekela maka - maka . Conco , mkhalidwe woipawu umene unali kucitika mu ulamulilo wa Aroma uonetsa kuti fanizo limene Yesu anakamba linali loona . Anthu akupitilizabe kuononga zacilengedwe mofulumila kwambili kuposa mmene dziko limadzibwezeletsela . Komabe , mofanana ndi Nowa , timaopa Yehova osati anthu . Ngati yankho lanu ndi lakuti inde pa mafunso onsewa , kodi ndiye kuti munasankhidwa kuti mudzapita kumwamba ? Koma tsiku limene nidzakasankha ya golide , ndiye kuti basi anthu adzaleka kunipanga coseketsa . Tifunika kuuzako “ m’badwo wam’tsogolo ” zinthu zocititsa cidwi za gulu la Yehova kapena kuti “ Ziyoni , ” ndiponso coonadi ponena za paladaiso wauzimu . — Ŵelengani Salimo 48 : 12 - 14 . Adzakuthandizani kuphunzitsa ana anu . Ndipo linakambanso kuti kumeneko kunali kufunikila anchito ambili . Kodi mungakhulupilile lonjezo laconco , mosasamala kanthu kuti likamba za munthu amene wafa lomba apa kapena za amene anafa kale - kale ? Kodi inu mwatsimikiza mtima kucita ciani ? Komabe , pali cina cake cofunika kwambili kuposa mkate kapena cakudya . The Harp of God Akristu odzozedwa amakono anakambilatu pasadakhale kuti 1914 cidzakhala caka capadela . Patapita caka cimodzi Victor Vinter anakukila ku Sokuluk . “ Kodi mfundo izi ndingazigwilitsile nchito bwanji pa umoyo wanga ? ” Mwacitsanzo , ganizilani nkhani ya kumwa moŵa . Timafunika kupeleka thandizo lakuthupi kwa anthu othaŵa kwawo , koma cofunika kwambili n’kuwathandiza mwauzimu ndi kuwalimbikitsa . Tiyeni tikumbukile kuti Paulo ndi ena a m’zaka 100 zoyambilila amene anakondweletsa Mulungu , anali kukhala na umoyo monga munthu aliyense . Ubatizo ndi cinthu cimene Mkristu aliyense ayenela kucita , ndipo ndi wofunika kuti tikapulumuke cisautso cacikulu . Iye anati : “ Zimenezo zinandidzidzimutsa kwambili . ” Kodi Mulungu amagwilitsila nchito mgwilizano wa zipembedzo kuti athetse mavuto padziko lapansi ? Kudzipeleka kwa Yehova ndi cosankha cabwino kwambili cimene munthu angapange . Kodi mumachula zinthu mwacindunji popemphela ? Wacicepele wina anati : “ Moyo wanga nidzaugwilitsila nchito kutumikila Mulungu . ” Patangopita miyezi yocepa , anadzipeleka kwa Yehova . Nanga munthu amadziŵa bwanji kuti wasankhidwa kuti adzapite kumwamba ? Iye anali kudalila kwambili Baibo ya Lefèvre pomasulila Malemba Acigiriki . Mwacitsanzo , ganizilani Yobu 26 : 7 . M’bale Nsomba ndi akazi ao a Lidasi ali kutsogolo kwa Nyumba ya Ufumu mu 2004 Mulungu anasankha Yesu kuti agwile nchito yotonthoza anthu . Buku lakuti All Things in the Bible linati : Abusa anali kulekanitsanso nkhosa pa nthawi ya “ kubeleka , kuyamwitsa , ndi kumeta ubweya . ” ( 2 Akorinto 7 : 1 ) Timapewanso zinthu zimene Baibulo limaletsa , monga kuledzela , ciwelewele , ndi kuba . — 1 Akorinto 6 : 9 - 11 . Bwanji osatsatila uphungu wa Yesu Khristu wakuti : “ Zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inunso muwacitile zomwezo . ” Dziŵani kuti Yehova amayamikila kwambili zimene mumacita pocilikiza ulamulilo wake mwa kum’tumikila mokhulupilika ndi kupilila ziyeso . Kutaya zonyansa za munthu . Mwina inu munaonapo mmene Yehova anakupulumutsilani na dzanja lake lamphamvu pamene munakumana ndi ciyeso . Nthawi zonse , Yehova amadalitsa zosankha zimene zimaonetsa kuti timam’dalila . Ndi zinthu zotani zimene zinacitika ku Yerusalemu mu 66 C.E . ? Kodi iye anaganizako zakuti asaulule zoipa zimenezo ndi colinga cakuti abale akewo amukonde ? Ufumuwo sudzapelekedwa kwa mtundu wina uliwonse wa anthu , koma udzaphwanya ndi kuthetsa maufumu ena onsewo , ndipo udzakhalapo mpaka kalekale . ” Baibo imati : “ Zonse zimene mukucita , muzicite mwacikondi . ” Iwo amadziŵa kuti nthawi yakwana yakuti abwelele kumalo kumene amaikila . “ Cishango cacikulu ” cimene msilikali waciroma anali kunyamula cinali ca makona 4 , ndipo cinali cacitali bwino , moti cinali kumuteteza kucokela m’mapewa mpaka m’mawondo . Mayankho anu pa mafunso amenewa angaonetse zimene mudzacite anthu akadzakupemphani kuti munenepo maganizo anu pa nkhani za mikangano . Ambili angavomeleze kuti n’zimene zinacitikadi kwa iwo . Nanga angasiyanitse bwanji cabwino ndi coipa ? ( 2 Pet . 3 : 3 - 7 ) M’malomwake , tiyenela kugwilizana ndi Akhiristu anzathu mwa kupezeka pa misonkhano nthawi zonse , cifukwa n’kumene kumapezeka mzimu wa Mulungu . 1 : 1 ) Abale na alongo a m’mipingo ya m’madela amenewa anali a zikhalidwe zosiyana - siyana . Makhalidwewo amaphatikizapo kulimbikitsa magaŵano , kukhalila mbali , kutengelana ku makhoti , kusagonjela umutu , ndi kukondetsa kudya na kumwa . M’citundu coyambilila cimene Baibo inalembewa , liu lakuti “ kumvela ” nthawi zambili limatanthauza ‘ kutsatila . ’ Mungayambe kucita zinthu ngati kuti muli kale ku dziko limenelo . Atate anamwalila ndili ndi zaka 6 ndipo zimenezi zinapangitsa kuti amai akhale ndi nchito yaikulu yotisamalila . ( Deuteronomo 6 : 6 ; 30 : 16 , 19 ) Koma n’zacisoni kuti anthu ambili asoceletsedwa mofanana ndi anthu oyambilila . — Ŵelengani Chivumbulutso 12 : 9 . Baibulo lionetsa kuti zinthu zidzaipilaipila ‘ m’masiku otsiliza . ’ ( 2 Tim . 3 : 1 , 13 ; Mat . Amunawo anali kusiya akazi okula nawo , mwina kuti akwatilenso acitsikana , ngakhale akunja . Zingakhale conco makamaka ngati mtima wathu wonyenga watisonkhezela kucita zosiyana . Kuonjezela pa kukulitsa cikondi pakati pathu ndi kupezeka pa misonkhano kuti tilimbitse mgwilizano wathu , tifunikanso kumapemphelelana . Luka , “ dokotala wokondedwa , ” anasamalila zosoŵa za Paulo ndi ena amene anapita kukatumikila mipingo yosiyanasiyana . — Akol . Ngakhale n’conco , maganizo akewo anaonetsa kuti sanali wodzikonda . Yesu Mukatelo , mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu . ’ Ndimapemphela usiku uliwonse ndipo Yehova amanditonthoza . ” Kodi Akhristu ena ambili aseŵenzetsa bwanji ufulu wawo mwanzelu ? Ndiponso , . . . ndidzabwelanso kudzakutengelani kwathu , kuti kumene kuli ineko inunso mukakhale kumeneko . ” — Yohane 14 : 2 , 3 . Ifenso tifunika kudzifufuza mofananamo . Tili ndi cidziŵitso colongosoka ca Mau ake ndipo timadziwa bwino coonadi conena za iye ndi zolinga zake . Cifukwa adzakhala atazoloŵela kale kugwila nchito . ” — Tara . Dalitso limenelo lipezeka pa Deuteronomo 30 : 19 , 20 . ( Miyambo 8 : 31 ) Mulungu anasankha anthu okwana 144,000 kuti akalamulile pamodzi ndi Yesu kumwamba . Yankho la Yesu linaonetsa kuti nthawi yakuti io adziŵe pamene Ufumu wa Mulungu udzayamba kulamulila inali isanakwane . N’ciani cimene mwamuna afunika kucita kuti nyumba yake ikhale malo abwino kapena a “ mpumulo ” kwa mkazi wake ? — Rute 1 : 9 . Tingacite ciani kuti zimenezo zisacitike ? Pamene mapeto a dzikoli akuyandikila , ifenso tikukhala m’nthawi yovuta . Onani masamba 215 mpaka 218 a buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni . Buku limeneli likupezekanso pa Webusaiti yathu ya www.jw.org . Kodi panakhala zotulukapo zanji ? Conco , ganizilani mmene Nowa anamvelela atadziŵa kuti dzina lake lili na tanthauzo lopatsa ciyembekezo . Cioneka kuti dzina lakuti Nowa limatanthauza “ Mpumulo ” kapena “ Citonthozo . ” ( Gen . Njila imodzi imene anacitila zimenezi ni kulandila uphungu kwa woimila Yehova , mneneli Natani . ( 2 Sam . 6 : 17 . Lefèvre anali kudziŵa bwino mmene ziphunzitso zabodza ndi maganizo olakwika a anthu zinakhudzila Chechi ya Katolika . Ngati mwaphunzila kugwilitsila nchito “ luntha la kuganiza ” mukali acinyamata , mudzakwanitsa kuyankha mafunso amene anzanu angakufunseni , monga akuti : ‘ Umadziŵa bwanji kuti kuli Mulungu ? ( Aheb . 11 : 7 ) Cigumula citatha , cikhulupililo cake cinamulimbikitsa kupeleka nsembe za nyama . Kuyelekezela Zinthu Kopindulitsa Kwambili 14 [ Mau okopa papeji 5 ] “ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi maganizo ako onse . ” — Mateyu 22 : 37 Kodi pali cifukwa colekela kukhululukilana ndi kupitiliza kutumikila Yehova mwamtendele ? ’ Ganizilani kuti mukuona Eliezere akufotokoza nkhani yonse kwa Betuele , bambo a Rabeka pamodzi ndi mlongosi wake Labani , ndipo io akumvetsela mwachelu . Nthawi zina anthu amanena zimenezi cifukwa cakuti anamva zimene ena amakamba . 6 : 1 - 3 . Kodi mau a Yehova ‘ anatsika bwanji ngati mame ’ ? Sitibadwa ndi cikhulupililo . A Yohane : Mukutanthauza ciani ? Salimo 72 : 16 : “ Padziko lapansi padzakhala tiligu wambili . Ndiye cifukwa cake mtumwi Paulo analemba kuti : “ Mau a Mulungu ndi amoyo ndi amphamvu . ” Iye anakamba kuti : “ Sinikayikila olo pang’ono kuti Yehova adzanisamalila . ” Atumiki ambili okhulupilika a Mulungu amamvela cimodzi - modzi . Kumeneko , iye anaphunzila citundu ca Cialubaniya , ndipo wathandiza anthu oposa 60 kuphunzila coonadi mpaka kubatizika . Kuti mudziŵe vuto la mwana wanu wacinyamata , mufunseni mafunso mokoma mtima ndiponso mwaulemu . Caciŵili , pamene Ahabu anauza Eliya kuti “ mdani wanga , ” anaonetsa kuti iye anali kudana ndi bwenzi la Yehova Mulungu , limene likanamuthandiza kusiya kucita zoipa . Quarrie ) , Na . Tikakumana ndi anthu otsutsa , kukhala waubwenzi kudzathandiza kuti tipewe mikangano ndi kutsegula mpata wakuti nthawi ina akatilandile mwaulemu . 2 : 8 , 11 ) Ndikali kukumbukila mau a m’bale wacikulile Saulo Teasi wa ku Tuvalu . M’nthawi ya atumwi , Yehova anadzoza Akristu ndi mzimu wake woyela . Ndipo ena anawapatsa mphamvu yocita zozizwitsa . Kodi ‘ Mudzakhalabe Maso ’ ? Ndalama zimenezi zimapelekedwa mwacindunji ku ofesi ya nthambi kapena kuikidwa m’kabokosi ka zopeleka kamene kali m’Nyumba ya Ufumu iliyonse . Mwina iye anaganiza kuti adzatuluka m’ndendeyo pamene Yehova anamuthandiza kudziŵa tanthauzo la loto la mkulu wa opelekela cikho ndi la mkulu wa ophika mkate . 17 : 1 , 2 , 16 ; 18 : 1 - 4 ) Zipembedzo zimenezo zidzawonongedwa kothelatu . “ Ukam’funafuna [ Yehova ] adzalola kuti um’peze . ” Dzina limeneli [ Yehova ] linali citetezo kwa Aisiraeli , ndipo linali ciyembekezo ndi citonthozo cao . ” [ Cithunzi papeji 10 ] ( Mateyu 5 : 33 ) Kodi mungaonetse bwanji kuti mumadziŵa kuti ndinu a Yehova ndipo mudzayamba kucita cifunilo cake nthawi zonse ? — Aroma 14 : 8 . 4 : 17 ; Mal . Gulu lake linafuula kuti : “ Amenewa ndi mau a mulungu , osati a munthu ayi ! ” Masiku ano , pempho limeneli lingaoneke lacilendo , koma m’nthawiyo zinali zofala mwamuna kutenga mkazi waciŵili , kapena cisumbali , kuti abeleke ana . NYIMBO : 96 , 94 Pamene mkazi wa Potifala anam’nyengelela kuti acite coipa , iye sanafune ngakhale pang’ono kucimwila Yehova . Zocita zathu pambali imeneyi zimaonetsa mmene timaonela dzina la Mulungu limene limalembedwa pa cikwangwani ca Nyumba ya Ufumu . — Yelekezani ndi 1 Mafumu 8 : 17 . Yesu anawayankha kuti : “ Onyenga inu ! Bwanji mukundiyesa ? ” Ngakhale masiku ano , Yehova amauzilatu anthu ake pasadakhale zimene zidzacitika mtsogolo . Yesu anakamba kuti tiyenela kupempha Yehova kutipatsa cakudya cimene tifunikila tsiku lililonse . Pamene Hillary Goslin anamvetselako nkhani imodzi , anabweleka galamafoni kwa mlungu umodzi kuti akauzeko anzake uthenga wa m’Baibulo . Ngati nthawi zina mumakayikila kuti Baibo imakamba zoona , onani vidiyo yaifupi yakuti Tingatsimikizile Bwanji Kuti Baibulo Limakamba Zoona ? Masiku ano , anthu amakonda kwambili ciwelewele , kumwa mwaucidakwa ndi zinthu zamalisece . Satana amafuna kusokoneza maganizo a anthu mwa kufalitsa mabodza . 2 : 21 ) Koma kodi zimenezo zinamukhudza bwanji Hana ? Yesu anakamba kuti iye ni “ mpesa weni - weni , ” Yehova ni “ mlimi , ” ndipo ophunzila ake ni “ nthambi . ” Munthu umafunika kusangalala na umoyo . ” Malinga ndi kauniuni wa ku France , hafu ya anthu kumeneko anakamba kuti amapemphela kapena kusinkhasinkha kuti “ amveko bwino . ” Kodi ufulu wathu wocita zinthu ungaonetse bwanji ngati timam’kondadi Yehova ? Akapolo ambili a ku Iguputo ndi ku Roma anali kucitilidwa nkhanza kwambili . Koma kuphunzila Mau a Mulungu , Baibulo , kwatithandiza kudziŵa anthu okana Kristu ndipo tamasuka ku cinyengo ndi mabodza a zipembedzo . — Yohane 17 : 17 . Komabe , Yesu anafotokoza momveka bwino kuti m’Cilamulo ca Mulungu kwa Aisiraeli munalibe ciphunzitso cotelo . Iye ndi mkazi wake anali kupanga bajeti ya zinthu zofunikadi . Koma pamene iye anali kukula anapitilizabe kukonda Mulungu . Mfumukazi Yezebeli inali kudziŵa kuti Malamulo a Mulungu amanena kuti pamafunikila mboni ziŵili kuti zitsimikizile munthu kuti wacita colakwa cacikulu . Ndiponso anali kuyembekezela kudzamanga nyumba ndi kukhalamo kapena kudzalima minda ndi kudya zipatso zake . N’cifukwa ciani tingakambe kuti Cingelezi ndi cinenelo codziŵika padziko lonse ? Iye anauza Yehova kuti : “ Sindine woposa makolo anga . ” Pitani kaseŵenzeni cabe . ” Ndikumbukila kuti Mboni za Yehova zinagogoda pacitseko maulendo ambilimbili , koma sindinatseguleko . ( Machitidwe 20 : 35 ) Kodi mukumbukila pamene munathandizapo munthu wina wosoŵa mwakuthupi ? ( Miy . 13 : 20 ) Mabwenzi auzimu adzakulimbikitsani kucita zabwino ndipo mudzatengela citsanzo cawo ca kudziletsa . Nchito imeneyi imacilikizidwa ndi zopeleka zaufulu za Mboni za Yehova . Iwo amatsatila malangizo a Yesu akuti : “ Munalandila kwaulele , patsani kwaulele . ” — Mat . Pamodzi ndi abale a m’mipingoyi , timagwila nchito yophunzitsa ena kuti ngati aonetsa cikhulupililo mwa Yesu , adzapeza moyo wamuyaya . ( Miy . 3 : 5 , 6 ) Pamene tiŵelenga Baibo ndi zofalitsa zimene gulu la Yehova limatipatsa , timadziŵa zimene zingatulukepo ngati sitinasankhe bwino . Izi zimatipangitsa kusankha mwanzelu . Anakambanso kuti : “ Popeza n’nali kukhala kutali ndi banja langa , nthawi zonse n’nali kudalila Yehova kuti anithandize . ( 2 Akor . 4 : 4 ) Tifunika kukhala ndi cikhulupililo ndiponso kuona zinthu ndi maso akuuzimu kuti tidziŵe zimene Ufumu wa Mulungu ukucita . NYIMBO : 63 , 59 Iye anafuna kuthandiza anthu ophunzila Ciheberi kusiyanitsa pakati pa mau a Ciheberi a m’Baibo oonetsa liu leni - leni ndi aphatikila ake a kumbuyo ndi a kutsogolo . Mainawa apezeka m’buku lochedwa Fivefold Psalter imene inatulutsidwa mu 1513 Petulo analoŵa m’cipinda cimene munaikidwa mtembo wa mzimayiyo poyembekezela kukauika m’manda . N’zomvetsa cisoni kuti Satana , mdani wamkulu wa Mulungu , akucititsa anthu kuika maganizo ao onse pa zinthu zakuthupi . Zimene mkulu angacite kuti akhale bwenzi la wophunzila zimasiyanasiyana malinga ndi cikhalidwe ca kumaloko . Komanso siticita nao zinthu zoonetsa kukonda dziko lathu . Ponena za odzozedwa , Informant inati : “ Cimwemwe cao cidzakhala cokwanila kokha ngati agwila nchito yocitila umboni za Ufumu . ” ( Aroma 4 : 11 ) Cikwati cawo cinali colimba , ndipo anali kulemekezana , kukambitsana bwino , ndi kukhala ofunitsitsa kuthetsa mavuto capamodzi . Koma copambana zonse n’cakuti iwo anali kudziŵika monga banja lokonda Mulungu . ( Mateyu 19 : 6 ) Ngati onse amakonda Yehova ndi kum’tumikila , banja lao limakhala lacimwemwe ndi logwilizana . Munthu akaona kuti maloto ake aja a zabwino sakwanilitsika onse , amakhala wosakhutila , kumva kugwilitsidwa mwala , ndi kukhumudwa . N’ciani cingatithandize kusankha mau abwino pokambilana ndi anthu ? Kodi tiphunzilapo ciani pa nkhani ya Rehobowamu ? Mulungu amatitsimikizila kuti “ amapeleka mphoto kwa anthu omufunafuna ndi mtima wonse . ” Mlongo wina wa ku United States anati : “ Kwa zaka zambili , ine na mwamuna wanga takhala tikuceleza abale obwela kudzakamba nkhani mu mpingo mwathu pamodzi na akazi awo . Kwa zaka zambili , aneneli a Mulungu anacenjeza Ayuda kuti ngati apitiliza kusamvela malamulo a Mulungu , adzapelekedwa m’manja mwa Ababulo . Nanga n’zinthu ziti zimene mungacite kuti mukonze cipulumutso canu ? Kuti ciwombankhanga ciuluke m’mwamba kwambili ndi kuyenda mtunda wautali , sicidalila mphamvu zake zokha . Kucita zionetselo zosakondwa sikunali kukhutilitsa khalidwe langa laciwawa . Yesu anati : “ Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha , kuti aliyense wokhulupilila iye asawonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” Yesu n’citsanzo cabwino kwambili pankhani imeneyi . Iye anati : “ Mupitilize kutelo mowonjezeleka . ” ( Machitidwe 20 : 35 ) Ndiponso , n’kocititsa cidwi cifukwa asayansi apeza kuti munthu wopatsa amapindula . 13 : 23 ) Conco , sitiyenela kuganiza kuti utumiki wathu suyenda bwino cifukwa cakuti nchito yathu siikubala zipatso . Iye anali kukonda kwambili ophunzila ake moti anapeleka moyo wake cifukwa ca io . Tikadziŵa mbali zimene siticita bwino , tiyenela kucitapo kanthu kuti tikule kuuzimu . Popeza kuti Mulungu sanganame , nikhulupilila kuti atate nidzawaonanso pa nthawi ya kuuka kwa akufa . ” — Mlaliki 9 : 11 ; Yohane 11 : 25 ; Tito 1 : 2 . ( b ) Nanga pangano la Cilamulo linali kudzateteza ciani ? Mulungu sayembekezela kuti tizikamba cinenelo cina cake kuti tim’dziŵe ndi kudziŵa zolinga zake Conco makolo angacite bwino kutengela citsanzo ca Mulungu pa nkhani ya kumvetsela pamene ana ao akulankhula . N’cifukwa ciani tifunika kulandila alendo ? Kodi pali nthawi ina imene munacita utumiki ngakhale kuti zinthu zinali zovuta ? Pakati pa anthu amene anacoka ku France kupita ku Poland kukalalikila uthenga wabwino m’mizinda ikuluikulu , panali Teofil , Piaskowski , Szczepan , Kosiak , ndi Jan Zabuda . Iye anagwilitsila nchito Aamaleki kuti akwanilitse colinga cake cimeneci cifukwa cakuti io anali adani a anthu a Mulungu . ( Num . Ndipo n’cifukwa ciani amakulalikilani panyumba panu ndi kumalo ena amene kumapezeka anthu ambili ? Panopa dzina la Yehova likupezeka m’Baibulo la Dziko Latsopano , ndipo Baibulo limeneli likupezeka m’zinenelo zoposa 130 . Zimenezo zinali zoopsa cakuti nthawi zina ndinali kunyamula mfuti . Caciŵili , sitiyenela kuganiza kuti anthu onse amene amabwela kudzasonkhana nafe kapena kuphunzila nafe Baibulo adzakhala a Mboni za Yehova . TSAMBA 7 • NYIMBO : 63 , 66 Anthu ambili masiku ano amapanga bajeti kapena kuika kandalama “ kenakake pambali ” kuti akaponye m’mabokosi a zopeleka za “ Nchito Yapadziko Lonse . ” 14 : 8 ; Sal . Pali anthu ena amene amaona kuti akhoza kuzindikila paokha matanthauzo a mfundo za m’Baibo . Buku lina limati : “ Umenewu unali umodzi mwa milili yoopsa kwambili imene inacitikapo . Mwakutelo , sitidzayembekezela Akristu anzathu kucita zinthu zimene sangakwanitse . Sitiyenela kuiŵala kuti naonso mwina akukumana ndi mavuto amene ife sitikuwadziŵa . Tsiku lina , anafunsa bambo wa chalichi ca Anglican kuti : “ Kodi cimacitika n’ciani munthu akamwalila ? ” Nkhani zakuti “ Kodi Zinangocitika Zokha ? ” Wosimba ni David Sinclair Mwamunayo anagwila mau a Yesu a pa Mateyu 24 : 14 . ” 20 : 29 . Ana athu anali atacoka pakhomo , ndipo kunali kovuta kupeza anthu acidwi kuti tiphunzile nao Baibo . Komabe , atsogoleli acipembedzo analephela kuletsa Mau a Mulungu kufalikila kwa anthu , amene anali na cifuno coŵelenga Baibo na kuimvetsetsa . Kodi ciyembekezo cinalimbitsa bwanji cikhulupililo ca Nowa ? Si conco ? Kodi nditumileko winawake uthenga umenewu ? Lomba nikutumikila monga mpainiya wanthawi zonse mumpingo wa citundu camanja , ndipo naphunzila kulalikila anthu a mitundu yonse . ” 16 : 18 ; Yes . Citsanzo coyamba cili apa pa 1 Mbiri caputala 29 vesi 26 ndi 27 . 23 Cilango Ni Umboni Wakuti Mulungu Amatikonda Mdani wao woipa kwambili wacikanani anathaŵa . Muyenela kuzitumiza limodzi ndi kalata yonena kuti zinthuzo ndi mphatso . Ndipo n’cifukwa ciani kukambilana zimenezo n’kofunika ? Buku lina linati : “ Anthu amene amakonda kuŵelenga ndi kulemba mabuku anaikonda kwambili njila imeneyi , ndipo pacifukwa cimeneci , Baibulo linafalikila kwambili . ” [ Mau apansi ] Yehova anatumiza angelo kukapha ana aamuna oyamba kubadwa aciiguputo . — Sal . N’zoona kuti palibe munthu wangwilo . Coyamba , tiyenela kutsatila malangizo a pa Miyambo 3 : 27 . Zoona , kuseli kwa cinthu ciliconse copangidwa mwaluso kuli munthu wanzelu . 3 : 6 ) Conco m’pempheni mzimu woyela , ndipo citani khama kuphunzitsa ana anu okondedwawo . Mukacita zimenezi , Yehova adzakudalitsani kwambili . — Aef . Iye anafa imfa yoŵaŵa . Abale ena amaganiza kuti apainiya apadela sasoŵa kanthu cifukwa cakuti amapatsidwa alawansi . ” M’malo mocitapo kanthu nthawi imeneyo , ndinamuuza kuti apite kucipinda cake , cifukwa ndinali nditakwiya kwambili cakuti sindikanapanga cosankha coyenela . Njila zimenezo zinali zothandiza kwambili makamaka panthawi imene kunali anchito ocepa . ( Aheberi 4 : 12 ) Amuna anga , a Bienvenido , amene anali wapolisi , anabatizidwa mu 1979 . Ndipo amai anga anamwalila atangoyamba kumene kuphunzila Baibulo . Inde Atate wanga , ndikukutamandani cifukwa inu munavomeleza kuti zimenezi zicitike . ” Munthu amene watsala pang’ono kumwalila afunika kum’tsimikizila kuti mumam’konda ndi kuti simudzam’siya . Conco , masomphenyawa ayenela kuti anawalimbikitsa ngako . Kodi mumpingo wacikristu timapezamo citetezo ndi citsogozo cotani ? 73 : 18 , 19 ) Mukayesedwa kuti mucite chimo , dzifunseni kuti , ‘ Kodi zimenezi zidzakhudza bwanji tsogolo langa ? ’ 15 , 16 . ( a ) Kodi Mau a Mulungu athandiza bwanji Akhristu kupewa mikangano ? Sitidzafunikila kuika cidalilo cathu pa dziko kuti tipeze thandizo . Zimenezo zinathandiza kuti anthu masauzande ambili athe kudya cakudya pa nthawi yopuma . 1 - 3 . ( a ) Olo kuti zinthu zikhale bwanji , n’ciani cimene tiyenela kuikako nzelu ? ( a ) Kodi tiyenela kukumbukila ciani cokhudza mmene zinthu zidzacitikila pa cisautso cacikulu ? Cotelo , muyenela kuyesetsa kulemekeza ndi kulimbikitsa abale ndi alongo okalamba mwa kulankhula mau olimbikitsa . Ndipo Baibo imafotokozanso zimenezi . Onani zimene imakamba . Mogwilizana ndi cenjezo la Inoki , Yehova anabweletsa cigumula camadzi cimene cinawononga anthu osaopa Mulungu m’masiku a Nowa . Ndipo abale othaŵa kwawo angaonetse mtima woyamikila ngati apewa kupempha - pempha . Izi zingacititse abale a m’dziko limene athaŵilako kuti aziwathandiza mokondwela . M’kupita kwa nthawi , Alexander Wamkulu anagonjetsa maiko ambili padziko lapansi , ndipo anthu ambili m’maikowo anayamba kukamba Cigiriki . ( b ) N’ciani cinacitikila Sara , mkazi wa Abulahamu , cimene iye sanali kuyembekezela ? Kodi zolinga zimene munthu amakhala nazo zimagwilizana bwanji na zimene zili mumtima mwake ? Kodi zinali bwanji kuti ayambe upainiya ? 1 : 5 . Kenako anamuonetsa ndalamazo , na kukamba monyadila kuti : “ Uyu ndiye mulungu wanga ! ” Koma madalitso ena anali m’tsogolo . Ngati titsatila malangizo a Yesu akuti tizipempha kuti ationjezele mzimu woyela , ndiye kuti ticita zinthu mwanzelu Mwacitsanzo , ganizilani Cynthia , amene tachula poyamba . Tiyeni tione zitsanzo ziŵili zotsatilazi . Kodi mudzakhalabe wokhulupilika kwa iye ndi kwa anthu ake ? Mzimayiyo anauka nthawi yomweyo , ndipo Petulo “ anamupeleka kwa ” Akhristu anzake “ ali wamoyo . ” Yehova sanasinthe zofuna zake . 146 : 9 ) Koma ngati pafupi pali mpingo wa cinenelo canu , mufunika kusankha kaya kukhala mumpingo wa cinenelo canu olo wa cinenelo ca m’delalo . N’ciani cimacitika ngati tilamulidwa ndi ( a ) ucimo ? 22 Mmene Timavalila Umunthu Watsopano ndi Kusauvulanso N’zosadabwitsa kuti ana a m’bale ameneyu anapita patsogolo mwa kuuzimu . Timoteyo anali ndi vuto la m’mimba . Mwina vutoli linabwela cifukwa ca madzi oipa amene anali kumwa . Ngakhale kuti anthu amagwilitsila nchito zinenelo zosiyanasiyana , n’cifukwa ciani limenelo si vuto kwa Yehova ? Koma Yehova anam’tsimikizila kuti sadzakhala yekha pamene anamuuza kuti : “ Ndidzakhala nawe . ” — Eks . Nanga ndani amene anali kudzakhala mbeu imeneyo ? Coonadi ca m’Baibo n’nali kucikonda kwambili , komanso n’nali kukonda kuciphunzitsako kwa ena . Nthawiyo , mpamene ulamulilo wotsatizana wa m’banja la mafumu a Cichainizi ochulidwa m’mbili yakale unayamba , komanso kutatsala zaka 1000 kuti cipembedzo ca Cibuda ciyambe m’dziko la India . — Onani bokosi lakuti “ Dziŵani Izi Ponena za Baibulo . ” Yehova analamula magulu ankhondo a kumwamba kuti awononge anthu oipa ndi kupulumutsa anthu olungama . 4 , 5 . ( a ) Kodi fanizo la pa 1 Akorinto 12 : 21 - 23 , limatithandiza bwanji kudziŵa mmene Yehova amaonela zofooka za anthu ? Koma imfa sithawika . Mtumwi Paulo analemba zimenezi m’kalata imene analembela Akorinto kuti anthu ena anali akali ndi moyo , kuonetsa kuti anthuwo akanacitila umboni pa zimene anaona ndi kumva zokhudza Yesu . — 1 Akorinto 15 : 3 - 8 . Kodi tingawalimbikitse bwanji maphunzilo athu a Baibulo kuti azipezeka pamisonkhano nthawi zonse ? Tizikumbukila kuti Yehova nthawi zonse amadziŵa atumiki ake okhulupilika , komanso kuti nthawi zambili amawadalitsa m’njila imene iwo sanali kuyembekezela . Pamene Paulo analemba za “ amene sali pabanja , ” moona mtima anavomeleza kuti : “ Ndilibe lamulo lililonse la Ambuye , koma ndikupeleka maganizo anga . ” — Mateyu 19 : 11 ; 1 Akorinto 7 : 25 . Koma tonsefe tikhoza kukhala monga amishonale mumpingo wathu . Anacita zimenezi kuti Davide asakhetse magazi . ( 1 Sam . Ataika malilo , Poli ndi mwana wake wa zaka 15 dzina lake Daniel , anasamukila ku Canada . 18 : 4 . Kusadziletsa kungabweletsenso mavuto monga ucidakwa , kukamba mau oipa , ciwawa , kusila kwa vikwati , nkhongole zosafunikila , zizoloŵezi zoipa , kumangidwa , kuvutika maganizo , matenda opatsilana mwa kugonana , mimba zapathengo , ndi mavuto ena ambili - mbili . — Sal . 4 : 2 ) Ngati munthu amacita bwino , amaonekela . — Ŵelengani 1 Timoteyo 5 : 25 . ( Mat . 1 : 25 ) Pamene zaka zinali kupita , Mariya anali kuganizila mosamala zimene zinali kucitika mu umoyo wa Yesu , ndiponso anali kumvetsela mosamala mau ake anzelu . M’nsapatomo anali kubisamo makope atsopano a Nsanja ya Mlonda . N’tayankha mafunso ake mopanda mantha kucokela m’Baibo , iye anakwiya n’kukamba mwaukali kuti : “ M’cotseni uyu . Mwacionekele , anthu a Mulungu anali kufunikila Baibulo lomasulidwa molondola ndi losavuta kumva . Kodi zimenezi zinam’phunzitsa ciani Mose ? Koma pamenepa iye anali kumvela Lamulo la Yehova lakuti Aisiraeli sayenela kugulitsilatu malo amene ndi colowa ca banja lao . ( b ) Ni funso liti limene tidzakambilana m’nkhani yotsatila ? Kuyambila kale - kale , anthu acikhulupililo akhala akuphunzila za Mulungu m’njila zitatu zikulu - zikulu . Yoyamba , mwa kuona cilengedwe cake . Yaciŵili , kuphunzitsidwa na anthu ena oopa Mulungu , ndipo yacitatu , mwa kudzionela okha ubwino wotsatila mfundo zake zolungama . ( Yes . Conco , n’zosavuta kukopeka na misampha imeneyi na kuyamba kuseŵenzetsa ufulu wathu molakwika . Amuna amenewo sanapite kukayendela dziko kapena kukafufuza zinazake . ( Aroma 15 : 4 ) Kodi mukanatsatila mfundo za m’Baibulo popanga zosankha zofunika kwambili monga zokhudza nchito , banja , kapena kulambila , ngati Mabaibulo a masiku ano anali ndi zolakwika zokhazokha ? Cikwati cake cinasokonezeka . Pofotokoza kusiyana kumeneku , Paulo analemba kuti : “ ‘ Palibe munthu amene anaonapo kapena kumvapo kapenanso kuganizapo zimene Mulungu wakonzela omukonda . ’ Zakalezo zapita . ” — Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . ( Genesis 40 : 16 - 19 ) Mofanana ndi atumiki a Mulungu onse okhulupilika , Yosefe analengeza mauthenga ocokela kwa Mulungu onsewa — uthenga wabwino komanso uthenga waciweluzo . — Yesaya 61 : 2 . Ana anu ndiwo maphunzilo a Baibulo ofunika kwambili . 15 : 28 ) Ngati tilankhula tili okwiya , tingakambe mau amene tingamve nawo kuipa pambuyo pake . Ngakhale n’telo , Ayuda okamba Cigiriki komanso Akristu anali kukhulupilila kuti Baibulo la Septuagint linali Mau a Mulungu . NYIMBO : 40 , 50 Munthu wina anamufunsa kuti : “ N’cifukwa ciani unabwela kuno ? Komanso kuyandikana kwa nyumbazo kungaimilenso mgwilizano umene mtundu wonse wa Isiraeli unali nao pa kulambila . Kukhala na cidziŵitso colongosoka kukanawathandiza kupanga zosankha mwanzelu . ( Sal . Enanso angaganize kuti alibe nthawi yophunzitsa munthu wina . 6 : 9 - 11 ) Timakonda Yehova na kum’dalila . Ndiye cifukwa cake mu umoyo wathu , timafuna kukhala okhulupilika kwa iye ndi kutsatila malangizo ake olembewa m’Buku lake lopatulika . Ku 124 Columbia Heights , kumene n’natumikila kwa zaka zambili Ngakhale pamene tizunzidwa , timayesetsa mmene tingakwanitsile kukhala moyo mogwilizana ndi mfundo ndi malamulo ake olungama . Polemba za Inoki komanso amuna ndi akazi ena okhulupilika , mtumwi Paulo anati : “ Onsewa anafa ali ndi cikhulupililo . ” Buku la Levitiko limagogomezela za ulamulilo wa Yehova . MU 607 B.C.E . , asilikali acibabulo motsogolelewa na Mfumu Nebukadinezara Waciŵili , anawononga mzinda wa Yerusalemu . Nthawi zina ziwiya za m’nyumba zingaipitsidwe ndi mankhwala akupha kapena zingakhale ndi uve . “ Pamene munalandila mau a Mulungu . . . simunawalandile monga mau a anthu ayi , koma mmene alilidi , monga mau a Mulungu . ” — 1 ATES . Mtumwi Paulo anafotokoza kuti : “ Mwa cikhulupililo , Inoki anasamutsidwa kuti asafe mozunzika , moti sanapezeke kwina kulikonse cifukwa Mulungu anamusamutsa . Pakuti asanasamutsidwe , Mulungu anamucitila umboni kuti akukondwela naye . ” Iwo anena kuti : ‘ Bwelani tiwafafanize kuti asakhalenso mtundu . ’ ” Akristu sayenela kucilikiza kapena kuloŵa m’zipani za ndale . Komabe aliyense payekha ayenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ndimacilikiza mokwanila makonzedwe a Yehova okhudza kulambila koona ? ’ Pitani polemba kuti MABUKU > MAVIDIYO . M’malo mokhumudwa , iwo ayenela kupitiliza kutumikila Mulungu mokhulupilika pa malo awo atsopano . ( Mac . 13 : 13 - 16 , 42 - 44 ) Tikakhala na mau olimbikitsa ouza munthu , n’kukhalilanji zii osawakamba ? Ndikali kukumbukila fungo la inki komanso kutentha kwa makinawo , zomwe zinapangitsa kuti nchito yosindikiza bukuli pa manja ikhale yovuta kwambili . Iye amakonda ulaliki ndipo ndi wakhama kwambili . 7 : 12 , 13 ) Pambuyo pa zaka zoposa 1,000 , lonjezo limeneli linakwanilitsidwa pamene “ mbeu ” kapena kuti mwana wa Davide anaonekela . Yoyamba , anthu amatha kudziŵa zinthu , kuonetsa cikondi ndi kulemekeza Mlengi . Ise sitinazengeleze . Ndipo mpingo waung’ono unakhazikitsidwa ku Hemsworth . 31 : 12 ) Ngati timam’kondadi Mulungu , kucita cifunilo cake sikudzakhala kolemetsa . Muziika zolinga zauzimu patsogolo ndipo muzidalila Yehova pa zocita zanu zonse . Komanso , Yehova akudalitsa alengezi a ufumu padziko lonse amene , mokhulupilika ndi modzicepetsa , amapeleka ndalama zocilikiza nchito zimenezi . — Luka 21 : 1 - 4 . KWA nthawi yaitali , anthu akhala akugwilitsila nchito mau akuti “ wokana Kristu ” pa zinthu zosiyanasiyana monga mafilimu ndiponso kwa anthu olamulila . ( Lev . 5 : 1 ) Komabe , ngati zolakwa n’zing’ono - zing’ono , tikhoza kuzithetsa popanda kuuzako wina aliyense , ngakhale akulu . Iye anati : “ Tsiku lija n’nali wokhumudwa ngako , cakuti n’natsala pang’ono kuphonya misonkhano . 24 : 3 - 8 . Izi zionetsa kuti njila yaikulu imene Mulungu amatithandizila ndi kutipatsa zosoŵa zauzimu , koma amatipatsanso zosoŵa zakuthupi . 18 Makolo — Thandizani Ana Anu Kupeza ‘ Nzelu Zowathandiza Kuti Akapulumuke ’ Makope a magaziniyi oposa 52,000,000 amasindikizidwa mwezi uliwonse , ndipo magaziniyi imafalitsidwa m’zinenelo 247 . Inde , Yesu anatisiila citsanzo . — Yoh . 13 : 15 . Ndiyeno makolo ake anayamba kukamba za Mulungu — Yehova Mulungu . M’caputa 11 ca Aheberi , mtumwi Paulo anachula mayeselo amene atumiki a Mulungu ambili osachulidwa maina anapilila . Mapazi awo ni omangidwa m’matangadza , ndipo misana yawo ikali kuŵaŵa cifukwa comenyewa . ( Mac . ( Salimo 25 : 14 ) Ana anu adzaona kuti mumawakonda ndi kuwalemekeza , ndipo sadzavutika kukambilana nanu ciliconse . Pamene mukucita phunzilo laumwini , mungacite bwino kupeza zifukwa zina zimene mungaonjezele pa ndandanda imeneyi . Gulu la Yehova limatilimbikitsa kutsatila malangizo a Paulo akuti : “ Tiyeni tiganizilane kuti tilimbikitsane pa cikondi ndi nchito zabwino . Cinanso , mungadzipeleke kuti muzitumikila m’Dipatimenti Yoona za Mapulani ndi Zomangamanga ndi kuseŵenzetsa nthawi yanu kumanga Nyumba za Ufumu . Nkhani ya mu Yearbook inati alendowo anayamikila , ndipo anaona kuti makatoniwo anali “ mabedi ofewa ndi othuma kuposa kugona pa simenti . ” ( 2 Sam . 12 : 1 - 14 ) Nayenso mtumwi Paulo anafunika kulimba mtima kuti apeleke uphungu kwa Petulo , mmodzi wa atumwi 12 , pamene anaonetsa khalidwe lokondela abale ake Aciyuda . ( Agal . ( b ) N’cifukwa ciani ana ena safuna kuphunzila citundu ca makolo awo ? Kodi poyamba colinga ca Mulungu cokhudza dziko lapansi ndi anthu cinali ciani ? ( Lev . 19 : 18 ) Tikamakamba nkhani inayake , ena akhoza kukhala kumbali yathu . Kodi tiphunzilapo ciani pa zimene Paulo anakamba zokhudza kulambila mwana wa ng’ombe ? ( Gen . 3 : 15 ) Mulimonsemo , pa nthawiyo Yehova analepheletsa zolinga na zoyesa - yesa za Satana ndi angelo opandukawo mwa kubweletsa Cigumula . Sauli anali kufuna kuti Yonatani adzakhale mfumu yotsatila osati Davide . Mu mzinda wa Sheffield , anali kucita lendi nyumba ina yaikulu , ndipo m’bale waudindo ndiye anali kuiyang’anila . Mu April 1967 , patapita caka cimodzi tinakwatilana , ndipo anatilola kupitiliza kutumikila m’dela . 8 : 12 . ( 1 Maf . 15 : 9 - 13 ) Iye analimbikitsa anthu kuti “ afunefune Yehova Mulungu wa makolo ao ndi kutsatila cilamulo . ” Kuposa kale lonse , ino ndiyo nthawi yofunika kumvela malangizo a Petulo akuti : “ Muzicelezana popanda kudandaula . ” Limeneli ni khalidwe lokondweletsa komanso lofunika limene silidzatha . — 1 Pet . Adzaphunzila kuti sayenela kubwelela m’mbuyo akapeza anthu opanda cidwi , koma kuti ayenela kuleza mtima ndi kupilila mu ulaliki . — Agal . 5 : 22 ; onani bokosi yakuti “ Kuleza Mtima N’kofunika . ” Popeza Mulungu ndi wamuyaya , kwa iye zaka 1000 zili ngati tsiku limodzi . Palibe umboni woonetsa kuti masiku ano Mulungu amaseŵenzetsa angelo kuthandiza anthu mozizwitsa , monga mmene anacitila kwa anthu ochulidwa m’Baibo . Mngelo anauza Danieli wolungamayo kuti adzauka “ pa mapeto a masikuwo . ” 39 : 17 - 20 ) Iye anakhala m’ndendemo kwa zaka pafupi - fupi 13 . Panthawiyo , Amai anadwala kaŵili mwakayakaya , ndipo pa maulendo onsewo ndinali kubwelela kunyumba kuti ndikawasamalile . Ndipo ena amaona kuti kusapatsa ena moni kapena kusayankha akatipatsa moni , n’kusoŵa cikondi kapena kupanda ulemu . Kodi nthawi idzafika pamene kuipa na kupanda cilungamo zidzasila ? Mboni za Yehova n’zokonzeka kukuonetsani m’Baibo yanu zimene mungacite kuti mukhale okonzeka pamene mapeto a okwela pa mahosi afika . N’cifukwa ninji mumafuna kukhalabe munthu woona mtima ? Cifukwa zidzathandiza abale onse obatizidwa kudziŵa kuti afunika kuphunzitsidwa kuti azisamalila maudindo mumpingo . Kodi kuganizila za Yehova kungatithandize bwanji kukhala wodzicepetsa ? Conco , iye anakambanso na akulu angapo za nkhaniyi , ndipo onse anamupatsa malangizo a m’Malemba . Malemba amakamba kuti mwamuna amakopeka na khalidwe labwino la mkazi wake popanda mau . Mofananamo , anthu ena amayandikila Mulungu cifukwa ca kudzicepetsa kwa anthu ake . — 1 Pet . Ndakhala mu utumiki wa nthawi zonse kwa zaka 14 . Pa zaka zonsezi ndakhala ndikuthandiza anthu kudziŵa zimene Baibulo limaphunzitsa ndipo posacedwapa mkazi wanga anayamba utumiki wa nthawi zonse . Yesu sanathetse vuto la munthuyo . Mtumwi Paulo anafotokoza kuti anzake ‘ anamuthandiza na kumulimbikitsa . . . m’kusoŵa kwake konse ndi m’masautso ake onse . ’ — Akolose 4 : 11 ; 1 Atesalonika 3 : 7 . Mofananamo , kuti tikhale na cimwemwe tiyenela kukhala na makhalidwe abwino , na kutsatila mfundo zabwino mu umoyo wathu . Tisamakaikile kuti Yehova amatikonda kwambili . — Ŵelengani 1 Petulo 5 : 6 , 7 . ( Mlaliki 9 : 4 ) Inde , zingatheke kusangalala pa ukalamba wanu ngati muli ndi maganizo oyenela komanso kukhala wofunitsitsa kusintha . Poyamba , tinali kugwilitsilila nchito bolopeni ndi pepala pa nchito yathu yomasulila . KODI mumamva bwanji mukaganizila za ukalamba ? Kugwilitsila nchito magazi mwanjilayi , kunali cizindikilo cakuti ansembe adzacita nchito zao mokhulupilika . 13 Malinga na Aroma 10 : 1 , 2 , ni zifukwa ziti zimene zinacititsa Paulo kusaleka kulalikila kwa anthu amene sanali kulandila uthenga wa Ufumu ? Yesu anadziŵa kuti ophunzila ake anali kufunikila malangizo owathandiza kukhala alaliki ogwila mtima , ndipo anawasonyeza mmene ayenela kugwilila nchito imeneyo . Patapita nthawi , mfumuyo inatumiza nthumwi zake ku Yerusalemu , pamodzi na gulu la asilikali kuti akalefule Ayuda na kuopseza Hezekiya kuti angodzipeleka m’manja mwawo . ( 2 Maf . Ŵelengani nkhani yotsatila . Anali kutumikila modzipeleka pamodzi na Paulo , ndipo kucita izi kunalimbitsa ubwenzi wawo . N’zoona kuti kucita ciwelewele n’kulakwa . Koma kusoŵeka kwa cikondi m’banja ndi kumene kumacititsa okwatilana ena kuyamba kukondana ndi munthu wina amene si mwamuna kapena mkazi wao . ( Miy . 5 : 18 ; Mlal . Kapena mungayambe upainiya . ( Ŵelengani Chivumbulutso 7 : 9 , 13 , 14 . ) Nehemiya anati Solomo “ anakondedwa ndi Mulungu wake , mwakuti Mulungu anamuika kukhala mfumu ya Isiraeli yense . Ndikusamalila ziwiya zotenthetsela m’maofesi ku Beteli ya ku Brooklyn Iye anakamba kuti : “ Mwamuna wanga anandiletsa kupita kumisonkhano ndipo anandiletsanso ngakhale kuchula dzina la Mulungu . Inde , cifukwa iye anati : “ Ndinapulumutsidwa m’kamwa mwa mkango . ” — 2 Tim . Yehova anacita zozizwitsa kuti atulutse anthu ake mu Iguputo ndi kugonjetsa mafumu ambili m’Dziko Lolonjezedwa . Onani nkhani yakuti “ Kodi Muli ndi Lamulo Loletsa Mavidiyo Ena , Mabuku Ena Ndiponso Nyimbo Zina ? Pambuyo pofotokoza fanizo la mpesa , Yesu anakamba kuti tikamagwila nchito yolalikila za Ufumu , tidzakhala acimwemwe . ANTHU ambili amakhulupilila kuti Mulungu alibe nazo kanthu zimene io amacita . 18 : 19 ; 19 : 1 - 4 . Vuto lina lalikulu limene Anita anakumana nalo linali kuphunzitsa ana ake zokhudza Yehova . Ni mmenenso zinalili kwa Akhristu oyambilila . ( Mac . ( Mat . 10 : 5 - 7 ; Luka 9 : 1 - 6 ; 10 : 1 - 11 ) Motsatila citsanzo cimeneci , Yesu amaonetsetsa kuti anthu onse amene amatengako mbali pa nchito yolalikila Ufumu , alandila malangizo ndi kutinso ali ndi zida zogwilitsila nchito n’colinga cakuti alalikile mofika pamtima . ( 2 Tim . ( Onani kabokosi ) Mwina mungaloŵeze ena mwa malemba amenewo pamtima . Zaka za posacedwa , abale audindo a “ nkhosa zina ” akhala akutumikila monga otsogolela bungwe la Society loona za malamulo komanso mabungwe ena a anthu a Mulungu . Izi zathandiza Bungwe Lolamulila kuika maganizo onse pa kupeleka malangizo auzimu ndi citsogozo . ( Yoh . 10 : 16 ; Mac . Koposa zonse , tidzaonetsa kuti timayamikila Mlembi wa Baibo , Yehova Mulungu . Imeneyo idzakhala nthawi yopeleka mphoto kwa anthu okhulupilika ndi yopeleka cilango kwa osakhulupilika . Mwacitsanzo , ganizilani mndandanda wa ziphunzitso zimene zinamveketsedwa bwino m’buku limene tachula m’palagilafu yapita . Akristu amene afuna kukwatila kapena kukwatiwa afunika kusamala ndi anthu amene amagwilizana nao . Palibe wina wamphamvu , wanzelu kapena wacikondi kuposa Mulungu wathu . 2 : 21 , 28 , 32 . Nditatsiliza maphunzilo anga a m’hotelo m’tauni ya Graz , amai anandilipilila ndalama zina kuti ndionjezele maphunzilo ena a m’hotelo . Mtumiki wodzipeleka wa Yehova komanso wotsatila Mwana wake mokhulupilika , ayenela kulemekeza nsembe ya Yesu . Angacite zimenezi mwa kupewa kudya zizindikilo za pa Cikumbutso ngati mumtima mwake sakutsimikiza kuti ndi Mkritsu wodzozedwa . Baibo imayankha momveka bwino kuti : “ Yehova ali pafupi ndi onse oitanila pa iye . Dzombe limodzi palokha silingacite zambili . Mwina mukudwala kwambili kapenanso muli ndi cisoni cifukwa cakuti munthu wina amene munali kumukonda anamwalila . Muzithandiza anthu pa zocitika za tsiku na tsiku . Kodi ndine wokonzeka kuphunzila cinenelo ca ku dziko limenelo ? Pelekani citsanzo . ( b ) Kodi fanizo limeneli likutiphunzitsa ciani ponena za Yehova ndi Yesu ? Tiyeni tikambitsilane mmene amacitila zimenezi . Mng’ono wanga analoŵa m’gulu la zigaŵenga ndipo inenso ndinayamba kugwilizana nao . Kuti mulithetse , mungafunike kuŵauza zinthu zina zokhudza inuyo . Onani nkhani yakuti “ Kulera Ana Obadwa ndi Matenda Ozerezeka , ” mu Galamukani ya June , 2011 . Kodi mungacite ziti , kapena kukamba mau ati amene angathandize aliyense wa inu kudzimva kuti amalemekezedwa ? Koma pamene mwasamukila mu mpingo wina , mufunika kuzika mizu yatsopano kuti mupitilize kukhala wolimba kuuzimu . Kodi mau akuti Yehova Mulungu wathu ni “ Yehova mmodzi ” atanthauza ciani ? Mwacitsanzo , pamene pulezidenti wa ku America anagamula tsiku la 30 May 1918 , kukhala lopemphelela mtendele , magazini ya Nsanja ya Mlonda inalimbikitsa Ophunzila Baibo kucita nawo mapemphelo amenewo . Dzina limeneli limathanthauza kuti “ Yehova Adzapeleka Zinthu Zofunikila . ” — Gen . 22 : 14 ; mau a munsi . ZIMENE YEHOVA WACITA KUTI TIYANJANENSO NAYE Kapena tingayesetse kumvetsa mfundo za m’Baibulo ndi kuona mmene zingatithandizile paumoyo wathu . 1 : 8 ) Kukhala na makolo amene amakonda Yehova na mtima wonse ni dalitso . Iye anauzidwa kuti : “ Uziliŵelenga ndi kusinkha - sinkha usana ndi usiku , kuti uonetsetse kuti ukutsatila zonse zolembedwamo . ” ( Yos . Tikukulimbikitsani kupemphela kwa Mulungu kuti akuthandizeni kumvela pamene iye akukukokani . Kodi makolo angathandize bwanji ana ao kuti akhale paubale ndi Mulungu ? ( Yakobo 1 : 13 ) Baibulo limatiphunzitsa kuti Mulungu anapanga anthu angwilo . Timadziŵanso zolinga zao ndi zimene akucita kuti akwanilitse zolingazo . Iye anali kuwakonda ndi kuceza nao . ( Yobu 2 : 3 - 5 ) Mwacitsanzo , abale athu ena , monga aja amene anaikidwa m’misasa yacibalo ya Nazi , anakumana ndi mavuto aakulu cifukwa ca cizunzo . Mulimonse mmene mumamvelela , nkhani ya amuna anayi okwela pa mahosi ni imodzi mwa nkhani zodziŵika kwambili za m’buku yotsiliza ya m’Baibo ya Chivumbulutso . Izi ni zina zimene ma IUD okhala na mahomoni amacita zowonjezela pa zimene ma IUD okhala na kopa amacita . Mafunso awa ayankhidwa m’nkhani yotsatila . Atafika kumeneko , anayamba kuuza atumwi zimene zinawacitikila . 6 : 1 - 8 ) Zimenezi zikucitikanso lelo lino . Danieli ? ( Aroma 12 : 2 ) Yehova amagwilitsila nchito gulu lake kupeleka malangizo a panthawi yake . Petra , amene ali na zaka za m’ma 80 , anati : “ Nimafuna kucita zinthu zambili , koma siningakwanitse . 28 : 5 . Koposa zonse , mungakhale otsimikiza kuti mudzakhala ndi mtendele wamaganizo ndi kulandila madalitso a Yehova . — Afil . Kodi umoyo udzakhala bwanji mavuto akadzatha ? Nkhani ino idzatithandiza kuyamikila ubwino wolankhula ndi Mulungu woona . Kodi tingatsanzile bwanji mtima wa Yesu woganizila ena ? N’nalimbikitsidwa kwambili kukhala ndi m’bale wauzimu amene anali wokonzeka kunithandiza . Pokamba za iye , wamasalimo waciheberi analemba kuti : “ Inu , amene dzina lanu ndinu Yehova , inu nokha ndinu Wam’mwambamwamba , wolamulila dziko lonse lapansi . ” Mwacitsanzo , ophunzila ake anali kudziŵa kuti ciwelewele n’coipa . Koma patapita nthawi , iwonso anaphunzila coonadi . Wosimba ndi Mayli Gündel ( 2 Tim . 3 : 1 - 5 ) Ndipo dzikoli lidzapitilizabe kuipilaipila cifukwa ulosi wa m’Baibulo unakambilatu kuti : “ Anthu oipa ndi onyenga adzaipilaipilabe . ” — 2 Tim . Tikalakwa , Yehova amapitiliza kutionetsa cikondi . Buku la Uthenga Wabwino wa Mateyu lidzapatsa anthu amene sanaonepo Baibulo mwai wonyamula ndi kuŵelenga mbali ya malemba opatulika imeneyi . N’ciani cingatilepheletse kupindula ndi cakudya cakuuzimu cimene Yehova amapeleka ? Kodi nimadalila Yehova na Yesu monga mmene n’nali kucitila pamene n’nadzipeleka kwa Yehova Mulungu ? ’ ( Mat . 24 : 14 ; 2 Tim . 3 : 1 ; Aheb . Iwo anakhala mumdima usiku wonse m’cipinda capamwamba ca nyumba yawo , imene inali itagumuka - gumuka . Conco , simuyenelanso kudziimba mlandu . Cimphepo camphamvu cocedwa Haiyan cinasakaza cigawo capakati pa dziko la Philippines mu 2013 . Panthawiyo , Sheryl , anali ndi zaka 13 zokha , ndipo zinthu zao zonse zinaonongeka . Mwacitsanzo , Leopold Engleitner anali Mboni ya Yehova yacangu ya ku Austria . Iye anamangidwa ndi asilikali a Nazi , ndipo anamutenga m’sitima kupita naye ku ndende yochedwa Buchenwald . Malinga n’zimene buku lina linakamba , mauthenga aconco “ ndi oipa , owononga , ndi osayenela . ” Koma pamene tikula zinthu zimayamba kuvuta paumoyo . Iye anati : “ N’nayamba kunyalanyaza zolinga zanga zauzimu . Iye anati : “ Cofufumitsa cacing’ono cimafufumitsa mtanda wonse . ” Coyamba , mzimu woyela unatsogolela olemba Baibulo kuti alembe ziyeneletso za akulu ndi atumiki othandiza . Pamene mukuyesedwa kuti mubise chimo lalikulu , kaya la mng’ono wanu kapena la mnzanu , mungacite bwino kutengela citsanzo ca Yosefe ndi kutsimikiza kuti mwaulula nkhaniyo kwa amene angafunike kuisamalila ndi kuthandiza wolakwayo . — Levitiko 5 : 1 . Makolo anga anali ndi ana 6 ndipo ndine waciŵili mwa anawo . Nanga ndimagonjela akulu a mpingo wathu ndi aja amene amayang’anila mipingo padziko lonse ? ’ Ngati timam’kondadi Mulungu , tidzayesetsa kupewa zosangalatsa zimene timadziŵilatu kuti iye amadana nazo , komanso ngakhale zimene tikuona kuti mwina iye angadane nazo . — Ŵelengani Mateyu 22 : 37 , 38 . M’malomwake , amakhalabe wokhulupilika kwa Mulungu akayesedwa . — Ŵelengani Aefeso 4 : 14 , 15 . 110 : 2 ) Popeza kuti Kristu ndi Mfumu Yankhondo yosagonjetseka , iye amachedwa “ wamphamvu . ” Iye anamagilila lupanga lake m’ciuno m’caka ca 1914 . Mmodzi wa angelowo anabwelezanso lonjezo la Mulungu kwa Abulahamu lakuti Sara adzabeleka mwana , apo n’kuti Sara sakuonekela . Anali m’hema wake kumvetsela . Atumiki onse a Yehova ali ndi mwai wapadela wouzako ena za ciyembekezo cimeneci . ( 2 Pet . ( b ) Kodi fanizo la Yesu linakwanilitsidwa motani pambuyo pa 1914 ? Iye anali paubwenzi wapadela ndi Yehova , amene anam’thandiza kucita “ zinthu zazikulu ” potsogolela Aisiraeli M’dziko Lolonjezedwa . — Deut . Poyamba , tinali kutumikila m’tauni ya Armagh , kenako tinakatumikila m’tauni ya Newry . ( Mac . 9 : 31 ) Mzimu woyela , umene ni mphamvu ya Mulungu yogwila nchito , ungathe kutitonthoza kwambili . Koma kodi mungayankhe bwanji ngati munthu wina wakupemphani kuti mumuuze umboni , wotsimikizila kuti lonjezo lakuti akufa adzauka , lingakwanilitsidwe ngakhale patapita zaka zambili ? Ngakhale kuti pali abale ocepa omwe amakamba cinenelo cimeneci , io analandilabe mphatso yamtengo wapatali imeneyo . KUCOKELA paciyambi ca cilengedwe , Yehova ndi Yesu akhala akugwila nchito mogwilizana . Tiyenela kuona ciphunzitso cakuti akufa adzauka kukhala cofunika ngako , olo kuti timayembekezela kuti tidzapulumuka pa cisautso cacikulu na kudzakhala na moyo pa dziko lapansi kwamuyaya . Paulo anagwilizanitsa mwayi umenewu ndi kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova pamene anauza odzozedwa anzake kuti : “ Cotelo , popeza tsopano tayesedwa olungama cifukwa cokhala ndi cikhulupililo , tiyeni tikhale pa mtendele ndi Mulungu kudzela mwa Ambuye wathu Yesu Khristu . Mwa ameneyunso , ndiponso cifukwa ca cikhulupililo , takhala ndi ufulu woloŵa m’kukoma mtima kwakukulu , mmene tilimo tsopano . ” Kamtsikana kena kanaona utsi wocokela pa fakitale inayake ukukwela m’mwamba ndipo unayamba kuoneka monga mitambo . KUYAMBILA kalekale atumiki a Mulungu akhala akudziŵa kuti kuphunzila kumapindulitsa . N’ciani cinacitikila ana a Adamu ? ( Aroma 1 : 14 , 15 ) Komabe , n’kwanzelu kupewa kucita ciliconse cimene cingakhumudwitse anthu m’gawo lathu . Mau amaloŵetsedwa pa kompyuta ndi kupanga mafaelo amene amatumizidwa ku nthambi zimene zimasindikiza mabuku kupyolela pa Intaneti . 4 : 2 ) Ngati mwakumana na zovuta , musabwelele m’mbuyo pokwanilitsa zolinga zanu . Iye akuti : “ Ndisanagone usiku uliwonse , ndimapita pa denga la nyumba yathu ndi kuyamika mokweza mau pa zinthu 5 zimene zandicitikila pa tsikulo . Tengelani Citsanzo ca Mabwenzi Apamtima a Yehova , Feb . Nthawi zambili kulimbikitsa ena kumaloŵetsamo kuwayamikila pa zabwino zimene acita . David Schafer Conco , anthu ambili amakhulupilila kuti dziko lathu linapangidwa ndi colinga . — Ŵelengani Yesaya 45 : 18 . M’malomwake , iye anaonetsa ulemu kwa Eliya mwa kupitiliza kucita zinthu mmene Eliya anali kucitila , ndipo zimenezi zinathandiza kuti aneneli anzake ayambe kumudalila . Koma mwamuna wakeyo afuna kuti mlongoyo akhale panyumba . Ngati mlongo wapita ndi m’bale wobatizidwa kukacititsa phunzilo la Baibulo , mlongoyo ayenela kuvala cakumutu . Anafunikanso kupeza ndalama zokwanila kuti asamalile banja lake . Mkazi wanga , Rose , nayenso anali wofunitsitsa kuphunzila Baibulo . N’ciani cingatithandize kuti tizilankhula momasuka ndi Bwenzi lathu lapamtima ? ( 1 Timoteyo 4 : 8 ) Ambili amaona kuti kucita maseŵela olimbitsa thupi nthawi zonse ndi kothandiza . Ndiponso , ndife otsimikiza mtima kugwila nchito yolalikila mwamsanga monga mmene Yehova akufunila . Kodi ndi anthu onse amene amavomeleza Yesu kukhala Wolamulila wao ? Mofanana ndi Mose , tatsala pang’ono kuloŵa m’dziko latsopano limene Yehova anatilonjeza . ( 2 Pet . Ngati mizu yake ikali bwino , mtengowu sulephela kuphuka . Yesu analosela za nthawi pamene “ mtundu udzaukilana ndi mtundu wina ” ndipo njala ndi milili zidzakhala paliponse m’dziko . [ Mau apansi ] Maina asinthidwa . ( Onani polemba kuti ZOKHUDZA IFE > MAFUNSO OFUNSIDWA KAŴILIKAŴILI OKHUDZA MBONI ZA YEHOVA ) Conco kuyambila nthawiyo , iye anayamba kukhala ndi umoyo wogwilizana ndi mfundo za m’Baibulo ndi kucita zinthu zokondweletsa Yehova . Timapindula ndi nzelu zao ndi kukhulupilika kwao . Atsogoleli Aciyuda anawonjezela malamulo awo m’cilamulo ca Mose . Nthawi zonse amatipatsa zimene tifunikila . ” Gerhard , mwamuna wina wa ku Germany , anati : “ Tikakhala ndi mavuto kapena tikakhumudwitsana , malangizo a m’Mau a Mulungu amatithandiza kukhala oleza mtima ndi okhululukilana . ” Ngati ndinu kholo , kodi nthawi zina mumaona kuti udindo wophunzitsa ndi kuumba ana anu kuti adzakhale amuna ndi akazi acikhulupililo ni nchito yovuta moti simungaikwanitse ? Kodi Yehova anatilenga ndi maluso anji apadela ? Iye anafunika cabe kuyembekezela zimene Mulungu anamulonjeza . 10 : 13 ) Sandra nayenso akuvutika ndi matenda osacilitsika . ANTHU AMAFUNA - FUNA CIKONDI . A Zimba : N’cifukwa ciani mukutelo ? Atumwi 12 a Yesu salinso padziko lapansi , koma atumiki ambili a Yehova akutengela citsanzo cao pa nchito yolalikila . Koma Christoph analoŵabe kilabuyo . ( Tito 1 : 2 ) Ndipo anauzila mtumwi Paulo kulembela Akhiristu oyambilila aciheberi kuti : “ Pitilizani kutipemphelela , pakuti tikukhulupilila kuti tili ndi cikumbumtima coona , popeza tikufuna kucita zinthu zonse moona mtima . ” — Aheberi 13 : 18 . Mwacitsanzo , mwamuna wina ku Turkey anati : “ Ndinacita cidwi kwambili cifukwa cakuti pa Nyumba ya Ufumu panali posamalidwa bwino ndi padongosolo . N’cifukwa Ciani Zoipa Zimacitikila Anthu Abwino ? — July - August 2 : 42 ) Panthawi ya cinzunzo , mgwilizano wao unaonekela kwambili cifukwa panthawiyo ndi pamene anafunika kuthandizana kwambili . ( Mac . Cosasinthasintha : Ngati mwauza mwana wanu kuti mudzamulanga akacita colakwika cina cake , muzisunga mau anu . [ Cithunzi papeji 11 ] MVETSELANI [ Cithunzi papeji 11 ] PEMPHELANI [ Cithunzi papeji 11 ] KAMBILANANI udindo wa akulu pothandiza munthu amene wacita chimo lalikulu ? M’mau ena , tingakambe kuti Yehova amationa kukhala atumiki ake kokha ngati tibala zipatso . Zoonadi , Ufumu wa Mulungu , kapena kuti boma , ndi limene lidzakwanilitsa colinga ca Mulungu padziko lapansi . — Mateyu 6 : 10 . M’banja lathu tinabadwa okwanila 8 , ndipo ine ndine woyamba . Dzinali limatanthauzanso kuti Mulungu angapangitse cilengedwe cake kukhala ciliconse cimene iye akufuna kuti akwanilitse colinga cake . ” Ndinali kupeza ndalama mosavuta pogwilitsila nchito njila zimenezi . Iye anati : “ Nimakondwela kutumikila Mulungu . Ni mafunso ati amene angatithandize kudzipenda ? Kukonda Yehova kumatilimbikitsa kupilila ciliconse cimene iye walola kuti cicitike . Kodi Yohane anaona kuti Gayo afunika kulimbikitsidwa kuti apitilize kukhala wolimba mtima ? Abale ena a mumpingo wathu anali atatumikilapo pa Beteli , ndipo ena anali kutumikilabe pa Beteli . “ Musalole kuti munthu aliyense . . . akumanitseni mphotoyo . ” — AKOL . Si kuti zopeleka zathu zifunika kucita kukhala zoculukilapo iyai . N’nafunika kuyesetsa kukhala wodzicepetsa ndi kuleka ciwawa . N’nali kutengela maganizo olakwika a anthu amene n’nali kuwaona m’mafilimu na anthu ena a m’dela lathu . Mwati adziŵa kuti tili ndi nkhawa ? ’ 27 : 17 ) Shan , amene tam’chula kale , anati : “ Nikumbukila kuti abale anali kunithandiza . Mulungu anapatsanso Adamu nchito yopanga dziko lonse lapansi kukhala paladaiso . Dziko la Harana kumene iye anabadwila , linali kutali kwambili kuloŵela kumpoto koma ca kum’mawa . Chivumbulutso 21 : 4 : “ [ Mulungu ] adzapukuta misozi yonse m’maso mwawo , ndipo imfa sidzakhalaponso . Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . N’zoona kuti ise sitingacite kukamba zimenezo . Koma maganizo olakwika amenewa angabyalidwe mumtima mwathu na kuyamba kukula . Amayi anaphunzila coonadi kwa amayi awo a Emma Wagner . Ngati tafedwa , tingakhale na cidalilo cakuti Yehova adzatithandiza . Nanga ndimacita zinthu mogwilizana ndi mfundo za m’Baibulo zimene ndimaphunzitsa ena ? — Aroma 2 : 21 - 23 . Davide ndi anyamata ake anali “ ngati khoma ” kwa abusa a Nabala ndi nkhosa zake . 1 : 8 ) Yesu anakonzekeletsa ophunzila ake kugwila nchitoyi mwa kuwathandiza kuona makhalidwe abwino mwa anthu a mitundu ina . 16 : 24 . 14 , 15 . ( a ) Tingapindule bwanji ndi fanizo la Yesu la zofufumitsa ? Kuleka kupeleka ulemu ku mizimu ya makolo n’kupusa . ” Mulungu analenga angelo kale - kale akalibe kulenga anthu . Osati mocita ufumu pa anthu amene ali coloŵa cocokela kwa Mulungu , koma mukhale zitsanzo kwa gulu la nkhosa . ” — 1 Pet . 5 : 2 , 3 ; ŵelengani 2 Akorinto 1 : 24 . Iye anali ndi akazi 4 , akazi ake enieni anali Leya ndi Rakele ndipo adzakazi ao anali Zelipa ndi Biliha . 8 Cikondi Mofananamo , Mulungu watipatsa Mau ake amene amafotokoza zocitika za padzikoli . Wamasalimo Davide anaimba kuti : “ Kwa ine maganizo anu ndi ofunika kwambili , inu Mulungu , ndipo ndi oculuka zedi . N’cifukwa ciani mphunzitsi wa Mau a Mulungu afunika kuzindikila kuti ubatizo ni ofunika kwambili kwa wophunzila aliyense ? Ndiponso , tisaiŵale kuti Yesu anati : “ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ” ( Mat . Ndiyeno muuzeni kuti mumawakonda kwambili makhalidwe amenewa . Rosie anakamba kuti , “ N’nali kuvutika maganizo kwambili cifukwa coganizila mavuto oopsa amene ningakumane nawo m’tsogolo . ” ( Salimo 77 : 12 ; Miyambo 24 : 1 , 2 ) Tikasinkhasinkha zimene timaphunzila zokhudza Yehova ndi Yesu , timapindula kwambili . Tonse ndife opanda ungwilo , conco tiyenela kuyembekezela kuti nthawi ina iliyonse munthu akhoza kukamba kapena kucita zinthu zimene zingatikhumudwitse . Victoria anati : Conco , ipempheleleni nkhaniyi . ” Koma iye ‘ adzapambana pa nkhondo yolimbana nao . ’ Koma maganizo aconco ndi oipa ndipo angasokoneze munthu . Anthu a ku Korinto anali kunena kuti : “ ‘ Ine ndine wa Paulo , ’ ena amati , ‘ Ine ndine wa Apolo , ’ enanso amati ‘ Ine ndine wa Kefa ’ , pamene ena amati , ‘ Ine ndine wa Khristu . ’ ” Zocitika zina monga Cikondwelelo ca Misasa m’masiku a Nehemiya inali nthawi yosangalatsa . ( Eks . 23 : 15 ; Neh . Stephanie analinso kukhala ndi umoyo wosafuna zinthu zambili . Zimenezi zinamuthandiza kuti asunge ndalama zina kuti zikamuthandize pamene akutumikila ku dziko lina . Zitsanzo zao zingatithandize kukhala olimba mtima . Nkhani zanu ndi citsanzo canu zinali kulimbikitsa ena , ndipo maulendo anu aubusa anali kuwathandiza kupilila mayeselo ao . Zimalalikilanso m’cinenelo ca Cingabere Satana amafuna kuti tiziika zinthu za Ufumu pa malo aciŵili mu umoyo wathu . — Mat . ( Mateyu 19 : 12 ) Nayenso mtumwi Paulo anakamba za Akhristu amene anasankha kutengela citsanzo cake cokhala wosakwatila “ cifukwa ca uthenga wabwino . ” — 1 Akorinto 7 : 37 , 38 ; 9 : 23 . Pamene Kenneth anali kupeleka pemphelo kuti ayambe kuphunzila , mayiyo anayambanso kulila . Kucokela pamene Yehova analosela za Mpulumutsi wa anthu , kwa Mulungu zinali monga kuti dipo limenelo lalipilidwa kale . Mulungu anadziŵa kuti cifunilo cake sicidzalephela . ( Gen . Kuganizila zamtsogolo kungatithandizenso kuti tisamakhale ndi nkhawa kwambili ndi mavuto amene tikukumana nao . Yefita analibenso mwana wina . Kodi iye anasunga lonjezo lake ? Kupela ufa wophikila mkate . Amuna anayi okwela pa mahosi angaoneke odabwitsa ndi ocititsa mantha . Koma sitiyenela kuwaona conco . 27 : 11 ) Mwina enanu amuna anu kapena akazi anu si Mboni , koma mumapitiliza kucita zinthu za kuuzimu . ▪ Khalani ndi Cikhulupililo Cosagwedela mu Ufumu Mwina mungakhale ndi vuto kumasukila anthu ocokela kudziko lina . Njila imodzi yofunika ni kuphunzila buku lakuti , “ Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu . ” Kuti mudziŵe zambili zokhudza utumiki wanthawi zonse wa M’bale Morris , onani Nsanja ya Olonda ya March 15 , 2006 , patsamba 26 . ( Aheb . 12 : 12 - 16 ) Mwa kucita ciwelewele , iwo akanakhala ngati Esau , amene analephela ‘ kuyamikila zinthu zopatulika , ’ cifukwa cocita dyela na zinthu zakuthupi . Kuti muthandize ena kukhala omasuka mu mpingo , dzifunseni moona mtima kuti , ‘ Sembe n’nali ku dziko lina , kodi nikanakonda kuti ena anicitile ciani ? ’ ( Mat . Mukaseŵenzetsa malangizo awo , mudzakhala monga dothi lofewa limene Yehova angaumbe mosavuta ndipo mudzapindula kwambili . Pamene dzikoli ‘ likuipila - ipila , ’ tingayembekezele zinthu zovuta kwambili kutsogoloku . ( 2 Tim . Ndi citsanzo cotani cimene Asa anapeleka kwa anthu a ku Yuda ? Ndinasangalala ndi mayankho omveka bwino a m’Baibulo . ( b ) Kodi ubatizo umatanthauza ciani ? ( Ŵelengani Luka 2 : 52 . ) Kodi Zakeyu anacita ciani kuti akhale woyenelela kuloŵa Ufumu wa Mulungu ? Kuonjezela apo , kudzela m’Cilamulo iye anaphunzila mmene ayenela kucitila zinthu ndi anthu ena , ngakhale amene anali kumuzonda . — Ŵelengani Ekisodo 23 : 5 ; Levitiko 19 : 17 , 18 . M’mau ena tingakambe kuti iye anafunikila ‘ kuleka kucita zosalungama . ’ Iwo amadziŵa kuti moyo umakhala waphindu ngati munthu ali paubwenzi wabwino ndi Mulungu . ( Agal . 6 : 2 ) Yehova amafuna kuti onse amene amam’lambila azimvela malamulo ofanana . Tikatelo , tidzaona kuti Yehova ndi weniweni kwa ife , ndipo nafenso tidzakamba kuti : “ Ndinkangomva za inu , koma tsopano diso langa lakuonani . ” Mavuto na zinthu zina zoipa zimacitika cifukwa anthu ena amasankha kucita zoipa — Yakobo 1 : 14 , 15 . Iye sanafune kuloŵa m’cipembedzo ciliconse cifukwa anali kuopa kunamizidwa . ( Yesaya 40 : 28 ) Mofananamo , kalata ya Yuda imanena kuti Mulungu wakhalako “ kucokela kalekale . ” — Yuda 25 . Zimenezi zathandiza ambili kusintha umoyo wawo , kukhala ndi cikhulupililo colimba , ndi kubatizika . Anthu a m’banja lathu . 3 Kodi Mukukalamila Udindo ? MMENE BAIBULO INATETEZEKELA : Ngakhale kuti Mfumu Antiyokasi inayesetsa kuononga Mabaibulo m’dziko la Isiraeli , panthawiyo Ayuda anali atafalikila kale m’maiko ena ambili . Mathayela a njinga yake atawonongeka , anapitilizabe ulendo wake ali n’cidalilo cakuti Yehova adzamutsogolela . Apainiya akhama okwana 10 anali kukhala m’nyumba imeneyo , ndipo anali kucita zinthu zauzimu nthawi zonse . Iye anali kukamba ndi anthu ake mokoma mtima , modekha , ndi mwacikondi . Iwo amakondwela ndi dzina lanu tsiku lonse . Cilungamo canu cimawakweza . ” — Sal . Kodi kukhulupilila Yehova kunam’thandiza bwanji kuti asamaope anthu ? * M’nkhani yapita , tinakambilana mmene tingatengele citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wodzicepetsa ndi wacifundo . N’ciani cimacitika munthu wocotsedwa akalapa ? Nanga pakhala zotsatilapo zotani ? Anabwelezanso kuti : “ khalanibe maso cifukwa simukudziwa tsiku kapena ola lake . ” — Mat . 24 : 42 - 44 ; 25 : 13 . Kodi tingakambitsilane naye bwanji nkhaniyi ? David , amene ni mkulu anati : “ Musadzidalile . ( Mika 2 : 12 ) Ndiponso , Yehova anakambilatu mwa mneneli Zefaniya kuti : “ Ndidzapatsa mitundu ya anthu cilankhulo coyela [ ca coonadi ca m’Malemba ] kuti onse aziitanila pa dzina la Yehova ndi kumutumikila mogwilizana . ” ( Zef . Mtumwi Paulo anawalembela kuti : “ Dzina la Mulungu likunyozedwa pakati pa anthu amitundu cifukwa ca inu . ” — Aroma 2 : 21 - 24 . Imakamba kuti : “ Yandikilani Mulungu , ndipo iyenso adzakuyandikilani . ” 11 : 1 ; Mat . 2 : 23 . * ( Yoh . 5 : 30 ) Mwa kukhalabe wokhulupilika mpaka imfa pa mtengo wozunzikilapo , iye anaonetsa kuti analidi ndi mzimu wodzimana . — Afil . Popeza kuti Yehova amakonda anthu kwambili , anatumiza “ Mwana wake wobadwa yekha ” kuti adzatifele . Pajatu iye anati , ‘ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ’ ” ( Mac . Iye anaonekela kwa Abulahamu ndi kumuuza kuti : “ ‘ Kweza maso ako kumwamba , uŵelenge nyenyezizo ngati ungathe kuziŵelenga . ’ Iye anakulila mumzinda wa Uri , ku Mesopotamiya . ( b ) Kodi tikuyembekezela ciani posacedwapa ? Koma kuteteza dzina la Yehova ndi anthu ake ndiye cinali cinthu cofunika kwambili kuposa mavuto amene anali kukumana nao . ( Miy . 18 : 1 ) Conco , dzipendeni kuti muone ngati ndimwe otetezeka ku mauthenga osoceletsa a Satana . Yakobo anali ndi ana ena 10 aamuna , koma anali kukonda kwambili Yosefe . Kodi io anacita motani zimenezo ? Pa usiku wakuti aphedwa maŵa , Yesu analamula ophunzila ake kukumbukila nsembe imene anali pafupi kupeleka . Dziko lokonda cumali , limalimbikitsa anthu mamiliyoni ambili kugula zinthu zambili kuposa zimene afunikila . Kodi muli pafupi kutsiliza sukulu ? Mwa ici , iye anapeleka citsanzo cabwino kwa otsatila ake onse . Auzeni kuti mumawanyadila ngati asankha kuika cifunilo ca Yehova patsogolo osati cuma kapena kuchuka . Onse sanali olambila Yehova , Mulungu wa Baibo . Ndipo pa zikondwelo zawo za masiku akubadwa panacitika zinthu zoipa kwambili . Dzina la Yehova limalemekezedwa tikateteza cikhulupililo cathu Iye anali kuŵelenga mobwelezabweleza nkhani imene tidzaphunzila ndipo anali kuŵelenganso Malemba m’Baibulo lake la zilembo za akhungu . Kodi zimenezi zimacitikadi ? Paulo anawonjezela kuti “ kukoma mtima kwakukulu koculuka [ kwa Mulungu ] ” kunaonetsedwa “ kudzela mwa munthu mmodziyu , Yesu Khiristu . ” ( Maliko 13 : 27 ; Mat . 24 : 31 ) Kusonkhanitsa kumeneku sikukutanthauza kusonkhanitsa koyamba kwa Akristu odzozedwa kapena kuwadinda cidindo comaliza . ( Mat . Nkhani zing’ono - zing’ono zimakula kukhala mavuto aakulu . ciwelewele ? Koma zambili zimene io analosela sizinacitike . Ifenso ndife odala masiku ano cifukwa ndise cabe amene timadziŵika na dzina la Mulungu . Kumeneko , tinali kudutsa m’mapili komanso kuyenda maulendo atali - atali . Ngakhale n’conco , cinali cosangalatsa kutumikila abale a m’madela akutali monga banja . Analola kuti ziyesedwe mwanjila imeneyi , monga mmene amalolela Akristu onse kukumana ndi mayeselo osiyanasiyana . Zovala zake zikununkhila bwino monga “ mafuta onunkhila , abwino koposa . ” Ndi zonunkhila monga mafuta a mule ndi kasiya amene anali kuwagwilitsila nchito pa kudzoza kopatulika ku Isiraeli . — Eks . Tate wina ku Australia anayenda ndi mwana wake wa zaka pafupi - fupi 10 ku miziyamu ( malo osungilako zinthu zakale ) . Anatengelapo mwayi womuthandiza kulimbitsa cikhulupililo cake mwa Mulungu ndi m’cilengedwe . Komabe , ife tili ndi cikhulupililo cakuti Yehova adzayankha mapemphelo athu opempha Ufumu wake kuti ubwele . Timoteyo ayenela kuti anali na zaka pafupi - fupi 20 kapena kupitililako pang’ono pamene mtumwi Paulo anamupempha kuti akhale mnzake woyenda naye . Masiku ano , timayamikila kwambili alongo ambili amene amadzipeleka ndi mtima wonse kuthandiza pa nchito yomanga yosiyanasiyana . Kuonjezela apo , iye amadalitsa kwambili anthu amene amadzipeleka ndi mtima wonse kuti apititse patsogolo kulambila koona ndiponso amene amathandiza kuti dzina lake liyeletsedwe ndi kuti colinga cake cabwino cikwanilitsidwe . Fanizo la matalente limene Yesu anakamba mu ulosi wake wonena za mapeto a dziko loipali , limatilimbikitsa kukhala okhulupilika . 4 : 6 - 8 . 5 : 13 ; 1 Akor . 40 : 28 . Pambuyo pake , Yakobo anabala Yosefe , mwana wake woyamba kwa mkazi wake wokondeka , Rakele . Ngakhale n’conco , Malemba amakambako za iye , ndipo amam’chula na dzina laudindo loyenelela . ( Luka 9 : 51 - 56 ) N’zokayikitsa kuti Yakobo na Yohane akanakamba mau aconco cikanakhala kuti mudzi umene unawakana unali wa kwawo ku Galileya . N’zoonekelatu kuti tsankho n’limene linawacititsa kukhala na cidani cimeneci . Didier , amene tam’chulapo kale m’nkhaniyi , anakamba kuti : “ Kutumikila ku malo osoŵa ni maphunzilo abwino amene amatithandiza kukonzekela umoyo wa m’tsogolo . ” Pamenepa , iwo anali kutamanda Mulungu Wam’mwambamwamba osati anthu . ( Ower . 24 : 14 ) Koposa zonse , tidzakhala na cimwemwe coculuka , cimene cimabwela cifukwa codziŵa kuti Yehova amatikonda , popeza iye amakonda onse amene ‘ amabala zipatso mwa kupilila ! ’ ▪ Yehova Akutsogolela Nchito Yathu Yophunzitsa Padziko Lonse Kodi mungakonde kum’citila ciani Yehova mukali wacinyamata ? ( b ) Acicepele angakonzekele bwanji kuteteza cikhulupililo cao ku sukulu ? 6 : 7 - 9 . Conco , zimene Yesu anacita mu utumiki wake zimasonyeza kuti amakonda mtundu wa anthu . ( Chivumbulutso 11 : 18 ; Miyambo 2 : 22 ) Limenelo lidzakhala dalitso lalikulu . Pamene Aisiraeli anaganizila kwambili za lipoti loipa la azondi 10 , io anayamba kudandaula za Mose ndi Aroni . Ni njila iti imene Elias Hutter anayambitsa pofuna kuthandiza anthu ofuna kuphunzila Ciheberi ? Ngati timakhulupilila mphatso ya dipo imene Yehova watipatsa cifukwa ca cikondi cake , timalimbikitsidwa kuyamikila mphatso imeneyi ndi kutengela citsanzo ca Yesu mosamala kwambili Yehova anati : “ Mafupawa akuimila nyumba yonse ya Isiraeli . ” 4 Yehova Amadalitsa Kwambili Anthu Ofunitsitsa Kupeleka Onetsani kukhulupilika kwanu mwa kuika masinapu ya mnzanu wa m’cikwati pa malo oonekela ku nchito ( Aroma 5 : 12 ) Mwa njila imeneyi , Mdyelekezi anakhala ndi “ njila yobweletsela imfa . ” Tsiku lotsatila , pambuyo pofunafuna , tinangopeza cabe kalavani yokhala na mabedi aŵili . Ndipo m’buku lonse la Danieli , timapezamo maulosi ena okhudza Ufumu wa Mulungu mu ulamulilo wa Mwana wake . Timakonda Yehova ndipo timafuna kum’kondweletsa . M’nkhani ino , tidzakambilana za Naboti , ndi za mkulu wina wokhulupilika wa mumpingo wacikhristu wa m’zaka 100 zoyambilila , amene analakwitsa zinthu zina . ( Mat . 28 : 19 , 20 ) Cifukwa ca nchitoyi , caka ciliconse anthu mamiliyoni amaphunzila Baibo , enanso masauzande amabatizika , ndipo mipingo yatsopano mahandiledi imapangidwa . Mkazi wake naye anati : “ Utumiki uliwonse wandithandiza kupita patsogolo . Mofanana ndi alaliki a m’nthawi ya atumwi , apainiya acangu amalimbikitsa mpingo . Kapena mumapempha ena kuti akuuzeni zocita ? Mtumwi Paulo atafotokoza za kulambila fano la mwana wa ng’ombe anati : “ Zinthu zimenezi zinakhala zitsanzo kwa ife , kuti ifenso . . . tisapembedze mafano , mmene ena mwa iwo anacitila . Mukadziŵa zimenezo , mufunika kucitapo kanthu ngati mmene Yosiya anacitila . Koma atamva zimenezo , ananditsekela m’cipinda . Iye anakhalabe ndi apongozi ake , a Naomi , ngakhale kuti anali okalamba . Kodi zingakhale kuti Mulungu alikodi ? Genesis caputa 5 - 9 Sikuti Bungwe Lolamulila ndi langwilo . Mabuku anai a Uthenga Wabwino amafotokoza bwino zozizwitsa zolimbikitsa cikhulupililo zimene Kristu anacita . Paulo anachula Akhristu a ku Roma amene anawalembela kalata kuti “ abale . ” Kodi zimenezo ndi zoona ? Ndi mapindu otani amene Kyung - sook wapeza cifukwa ca mapemphelo amenewo ? Mwacitsanzo , mudzakhala ndi mipata yambili yoonetsa kuti mumakonda Yehova ndi anthu . Mudzakhalanso ndi mipata yoonetsa kuti mumayamikila kwambili ciyembekezo ca moyo wosatha . N’ciani cingayambitse ‘ mafunso opanda nzelu ’ ? Iye anati : “ Moyo ndaukana , sindikufuna kukhala ndi moyo mpaka kalekale . ” Yesu anapatsa ophunzila ake citsanzo pa nchitoyi . Atangobatizika , iye anayamba kulalikila za “ ufumu wakumwamba . ” ( Mat . Panthawi ina , mngelo analimbikitsa Danieli , “ munthu wokondedwa kwambili , ” kuti akhale na “ mtendele ” ndi kuti akhale “ wolimba mtima . ” — Dan . M’zaka za zana loyamba , Mulungu anatuma wophunzila Filipo kukakumana ndi nduna ya ku Itiyopiya ndi kukambitsilana naye tanthauzo la maulosi a m’Baibulo amene ndunayo inali kuŵelenga . Ambili amakonda kuceza pa Intaneti , kutuma mauthenga , kumvetsela nyuzi kapena kufufuza za maseŵela . Nanga mungakhale motani munthu wofikilika ? Izi zinanipatsa mwayi wotsatila mosamalitsa mapazi a Khristu , amene anali kupita ku midzi na mizinda yakutali , kukathandiza nkhosa za Yehova . Mosakayikila , ziyembekezo zimene anthu anali nazo zokhudza Mesiya n’zimene zinacititsa kuti anthu a ku Galileya aganize zolonga Yesu ufumu . Nkhaniyo imati : “ Mose anacitadi zomwezo , pamaso pa akulu a Isiraeli . ” 4 : 18 ) Koma tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ndimayendela limodzi ndi gulu pakakhala kusintha kwa kamvedwe ka mfundo za m’Malemba ? Iye anati : “ Ulamulilo wonse wapelekedwa kwa ine kumwamba ndi padziko lapansi . ” Onsewa amalambila Yehova mogwilizana ndipo apanga “ khamu lalikulu la gulu lankhondo . ” — Ezekieli 37 : 10 ; Zekariya 8 : 20 - 23 . Ngati n’conco , mungacite bwino kutengela citsanzo ca Timoteyo . Yehova anaika Adamu ndi Hava m’paladaiso . 1 - 3 . ( a ) Ni vuto lanji limene acicepele onse amakumana nalo ? Fotokozani fanizo . Ni “ uthenga wabwino ” uti umene Paulo anali kulalikila ? Nanga uthengawo unaonetsa bwanji kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova ? 45 : 16 ) Iwo azidzayang’anilidwa ndi Khristu ndi olamulila anzake okwana 144,000 . Ngati tikuvutika ndi matenda kapena mavuto ena amene sitingawathetse , tiyenela kum’tulila Yehova nkhawa zathuzo , podziŵa kuti adzatisamalila . ( 1 Pet . Mwacitsanzo , iye anali kunyamula Carol pa galimoto ndi kum’pelekeza kumene wafuna . Anali kumuthandizanso kugula zinthu ndi kumucitila zinthu zina zambili . 2 : 15 . Kuti timve zambili pa zocitika zolembedwa mu Oweruza caputa 4 tifunikanso kuŵelenga caputa 5 , cifukwa caputa cina cimafotokoza mfundo zimene m’caputa cinzake mulibe . ( b ) Ndi mfundo za m’Malemba ziti zimene mkulu angakambilane ndi m’bale amene safuna kukalamila maudindo ? 24 : 45 ) Yesu wakhalanso akugwila nchito mwakhama yoyenga anthu a Mulungu na kuwathandiza kuti kulambila kwawo kukhale koyela . — Mal . Iye analibe zinthu zambili . Analibe nyumba kapena malo . — Luka 9 : 58 ; 19 : 33 - 35 . Conco , inu mukutengako mbali mokwanila pa nchito yofunika imeneyi . ” ( a ) Kodi fanizo la Msamariya wacifundo tinali kulifotokoza bwanji ? Kodi n’ciani camuthandiza kupitiliza utumiki ? Kucoka nthawi imeneyo , ndinaona kuti Mboni ndi zosiyana ndi anthu ena . Kodi masomphenya a Zekariya ayenela kutikhudza bwanji masiku ano ? Tinali monga “ akapolo a zonyansa ndiponso akapolo a kusamvela malamulo . ” ( Salimo 36 : 9 ) Ndiye cifukwa cake m’pomveka kuti iye adzaukitsa akufa . Buku yakuti The Jewish Encyclopedia inati : “ Ayuda anayamba kukhulupilila kuti mzimu sukufa pambuyo potengela maganizo a Agiriki , makamaka cifukwa ca ciphunzitso ca Plato . ” Satana ndi “ wopha anthu , ” monga mmene Yesu anakambila . ( Yoh . ( Miy . 22 : 6 ; 27 : 11 ) Makolo angakhomeleze mfundo zabwino za Mulungu wathu woyela mwa ana awo . Munthu akhoza kusintha . Pamene n’nali wacicepele sin’nali kucikonda kweni - kweni coonadi . Kodi sindidzawaonanso ? ’ 2 , 3 . ( a ) N’cifukwa ciani kulimbana ndi zilakolako zoipa n’kofunika kwambili ? ( Mat . 6 : 30 - 34 ) Mau amenewa aonetsa kuti tiyenela kukhala okhutila ndi zinthu zofunika za tsiku ndi tsiku zimene tili nazo m’malo mofunafuna cuma . Mu ofesi yanga muli zithunzi zambili zimene ndimakonda . Mwacitsanzo , Naboti anakhalabe wokhulupilika ngakhale kuti anazunzidwa ndi kuphedwa . Kuti tiphunzitse cikumbumtima cathu ndi kucigwilitsila nchito , tifunika kucita zambili kuposa kungophunzila Baibulo . Munthu ameneyo anali Goliyati . Masiku ano , kupita patsogolo m’zamankhwala kwathandiza madokota kugwebana ndi matenda pofuna kutalikitsako moyo . Anthu amene anali kunyumba kwa mtsikanayo “ anali kudziŵa kuti wamwalila . ” N’ciani cinamuthandiza kukhala wacimwemwe ? 139 : 23 , 24 ; Yak . N’nacita zimenezi kuti n’satayenso mtendele wamtengo wapatali umene n’naupeza . ” Mtendele wa Mulungu unali kuteteza mtima wanga nikapemphela kwa iye tsiku lililonse . ( Mat . 6 : 19 - 21 ) Lomba tiyeni tiŵelenge ndi kupenda lemba la Mateyu 6 : 25 - 34 . Tikalola kuti coyamba timvetsele zimene mwana akufotokoza , nthawi zambili zotsatilapo zinali kukhala zabwino . ” 4 : 24 ; Akol . 3 : 10 ) Amakamba za umunthu umene “ unalengedwa mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu . ” Mosiyana na anthu amenewo , Yesu ‘ anaukitsidwa kwa akufa , ndipo sadzafanso . Mbalame zophiphilitsila zimenezi zimaimila anthu a mitima yabwino amene amapeza cakudya cakuuzimu , mthunzi , ndi malo okhala mkati mwa mpingo wacikristu . — Yelekezelani Ezekieli 17 : 23 . Ngati izi sizinathandize , mwina mungafunike kutsatila malangizo a pa Mateyu 18 : 15 . Kuwonjezela pa kudziŵa cinenelo catsopano , amene atumikila ku gawo la cinenelo cina , afunika kuonetsetsa kuti akudya cakudya cotafuna ca kuuzimu . ( 1 Akor . Magazini imeneyo inakamba kuti vutoli kwa ena lili monga “ munga m’thupi . ” Kodi Yehova anam’dalitsa bwanji Yosefe ? N’nadzifunsa kuti : ‘ Nidzamuuza ciani pakuti zonse azidziŵa kale ? 59 : 1 . Mu 1997 , M’bale ndi Mlongo Pierce anayamba kutumikila pa Beteli ya ku United States . Kapena muli mu utumiki , ndipo mwininyumba wakuuzani kuti , “ Ndine wotangwanika . ” 30 : 14 ) Makala onyamulidwa mwa njila imeneyi anali kuwayatsila moto poseŵenzetsa tunthyonthyo nthawi iliyonse paulendo wautali . Ayuda ambili anafika mpaka poumilila kuti Yesu aphedwe . Mau a Mulungu amayankha kuti : “ Bzala mbewu zako m’mawa , ndipo dzanja lako lisapume mpaka madzulo , cifukwa sukudziŵa pamene padzacite bwino , kaya pano kapena apo , kapena ngati zonsezo zidzacite bwino . ” ( Mlal . ATHANDIZENI KUPITA PATSOGOLO Tiyenela kucita ciani kuti tithandize ena kupita patsogolo ? Kaya ndife Akristu odzozedwa kapena a khamu lalikulu , Yehova watilonjeza tsogolo labwino . Mpaka muyaya ? ” Cifukwa cokhala opatsa , nthawi zambili amapeza zoculuka zimene sakanagula na ndalama — anthu amawakonda , na kuŵalemekeza , ndipo amakhala na mabwenzi abwino amene naonso amapatsa moolowa manja ! — Luka 6 : 38 . Kodi Baibo yakhalapobe mosasamala kanthu kuti panali zovuta ziti ? Iye anayembekeza “ kufikila nthawi ina yabwino . ” Ciŵelengelo ca anthu opezeka pa Cikumbutso ku Pittsburgh cinali kukwela caka ciliconse . Kwa zaka zambili , ndaona mmene Atate wathu wakumwamba Yehova , amasamalilila zosoŵa za anthu m’zinenelo zonse , mosasamala kanthu kuti cinenelo cao cimakambidwa ndi anthu ocepa kapena ambili . ( Sal . Iye ndiye “ Mwanawankhosa wa Mulungu amene akucotsa ucimo wa dziko . ” ( Yoh . Paulo anauza Akhristu anzake kuti ‘ acititse ziwalo za thupi lawo . . . kukhala zakufa , ’ kutanthauza kuthetselatu zilako - lako zonse zoipa zokhudzana ndi “ dama . ” Conco , ananditumiza kunyumba ya masisitele ku Madrid ndipo Lauri anamutumiza ku Valencia . Ku Micronesia , kuli mipata yambili yoyambitsa maphunzilo a Baibulo . Ndipo mukhoza kudzionela nokha mmene anthu amene aphunzila Mau a Mulungu ndi kuwagwilitsila nchito akupitila patsogolo . Mulekeni apite ! ” Cimene cinam’thandiza ndi kukumbukila cikondi cimene wokondedwa wake anali kumuonetsa kuti “ cimaposa vinyo kukoma kwake , ” ndipo dzina lake linali “ ngati mafuta othila pamutu . ” ( Ŵelengani 1 Timoteyo 5 : 4 , 8 ; 6 : 6 - 10 . ) A Mboni atabwela kudzaceza ndi mkazi wanga , ndinawafunsa kuti : “ Kodi Mulungu angandikhululukile macimo anga onse ? ” Kodi ubatizo wao umagwilizana ndi kuyeletsedwa kwa ana a Aroni ? Iyai . Kodi mau amenewa atiphunzitsa ciani za munthu wolungama ameneyu ? Ndinayamba kulila ndipo ndinalephela kupuma bwinobwino . Ndinali kuzimvela cisoni , koma zimenezi zinasintha nditafika zaka 14 . Ngakhale zinali conco , cifukwa ca cikhulupililo , iye anagwilabe nchitoyo . Umu ndi mmene iye anali kukambila zikomo . Kukamba zoona , pali zambili zimene tingaphunzile ku mbalame . Mungamuthandizenso kuganizila mmene kucita zimenezi kudzapindulitsila okalamba . Koma kodi mumalola mapulogalamu a pa TV , maseŵela a pa vidiyo , maseŵela olimbitsa thupi , ndi zimene mumakonda kusokoneza kupita kwanu patsogolo kuuzimu ? Ngakhale tili ndi cakudya cokwanila , tingacite bwino kuganizila abale amene ali pa umphawi kapena amene akukumana ndi zovuta zina . Ndi zinthu ziti zimene muyenela kucita kuti muzikhulupilila kwambili Yehova ndi kulimbitsa ubwenzi wanu ndi iye ? M’dziko la Germany , Ophunzila Baibulo oposa 20 anakanilatu kuloŵa usilikali , ngakhale kuti boma linakhwimitsa lamulo lokhudza ufulu wa anthu . M’nthawi ya Mose , Yehova anapatsa anthu ake malangizo omveka bwino pankhani ya makhalidwe ndi kulambila . Mu 1932 , Bulletin inati Akristu sayenela kukhala “ Oyela Mtima a pa Cikumbutso , ” omwe anali kudya zizindikilo koma n’kulephela kukhala “ anchito enieni ” olalikila uthenga wa coonadi . Kuyambila pamene anapanduka , Satana wakhala mdani wamkulu wa Yehova ndi anthu . Zipembedzo zimene zimatsatila maganizo a anthu n’zopanda phindu . — Maliko 7 : 7 , 8 . Pitani kakhwimitseni citetezo monga mmene mukudziŵila . ” Tonse timafuna kukhala ndi thanzi labwino kuti tizisangalala ndi umoyo ndiponso kuti tizitumikila bwino Yehova . Malinga ndi mau a Yesu , tiyenela kudzifunsa kuti , ‘ Ngati ndakumana ndi mavuto amene mnzanga akukumana nao , kodi ndingafune kuti ena andicitile ciani ? ’ Kaya iye anayankha molondola kaya . Nikhulupilila kuti anatelo . ” ( Aroma 5 : 12 , 15 , 17 ) Cisomo cimeneci cinabweletsa madalitso ku mtundu wa anthu . Ngakhale lomba , anthu amene ni mabwenzi a Mulungu angakhale na “ mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse . ” — Afilipi 4 : 6 , 7 . NYIMBO : 79 , 140 Koma mwadzidzidzi panabuka citsutso coopsa . Paulo anakamba mosapita m’mbali pamene analembela Akristu anzake aciheberi . Kupyolela mwa Mfumu Davide , Yehova anaulula kuti adzacita pangano ndi Yesu lokhala ndi zolinga ziŵili : Coyamba , kuti ‘ akhale kudzanja lamanja [ la Mulungu ] ’ kufikila atagonjetsa adani ake . Caciŵili , kuti akhale “ wansembe mpaka kalekale monga mwa unsembe wa Melekizedeki . ” Komabe , abale na alongo okhulupilika amene anatumikila Mulungu kucokela mu 1914 mpaka 1918 , pambuyo pake iwo anafotokoza momveka bwino kuti monga gulu , anthu a Ambuye anali okangalika pa nchito yolalikila kuti isalekeke . Nthawi zina nkhosa imatengeka ndi msipu ndi kuyamba kucoka pagulu pang’onopang’ono mpaka kutaika . Kodi ni mfundo ziti kapena makhalidwe ati amene tiyenela kukhala nawo kuti tipeze cimwemwe ? Atatsala pang’ono kukhazikitsa pangano latsopano , Yesu anapeleka malamulo aŵili ofunika kwambili . Pelekani citsanzo cosonyeza kusiyana pakati pa cidziŵitso , kumvetsa zinthu , ndi nzelu . ( Genesis 1 : 1 ) Limatiuzanso mmene dziko lapansi linalengedwela kuti pakhale zamoyo , mmene zamoyo zosiyanasiyana zinakhalilapo , ndiponso kulengedwa kwa anthu . Onani mau a m’kalata yake yoyamba yodziŵika ndi dzina lake . Mauwo amati : “ Ana inu , ino ndi nthawi yakumapeto , ndipo monga mmene munamvela kuti wokana Kristu akubwela , ngakhale panopa alipo okana Kristu ambili . Cifukwa ca zimenezi timadziŵa kuti ino ndi nthawi yakumapeto . Kukamba zoona , Yehova amatikonda ndipo afuna kutiteteza . 5 : 1 . N’cifukwa ciani tifunika kudalila mau a Yesu a pa Mateyu 6 : 33 ? Koma Adamu analibe “ womuthandiza . ” Komabe , n’kutheka kuti Marita anamvela zimene Yesu anacita . Patapita wiki imodzi , Luigi anapita kukacita ulendo wobwelelako kwa mayi wina . Iye anadabwa kuona kuti mwamuna wa mayiyo ni dilaiva uja amene anamunyoza . ( Salimo 49 : 7 , 8 ) Tifunikiladi thandizo cifukwa sitingakwanitse kulipila mtengo wa dipo . N’ciani cimene anthu ambili akamba ponena za Baibulo la Dziko Latsopano la m’zinenelo zao ? Pamene anakwanitsa zaka 16 molumikizila miyendo yake munaguluka , cakuti anafunika kucitidwa opaleshoni m’ciuno . Kodi nzelu n’ciani ? Nanga n’cifukwa ciani sitingakambe kuti kuculuka kwa zaka ni umboni wakuti munthu ali na nzelu ? Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti sanafune kutengako mbali m’mikangano ya ndale ? Rose anazindikila kuti palinso njila zina zoŵelengela Baibo . POFUNA kuyesa Yesu , Mfarisi wina anam’funsa kuti : “ Mphunzitsi , kodi lamulo lalikulu kwambili m’Cilamulo ndi liti ? ” Ngati wocimwa wathaŵila kwa Khristu mwa kum’khulupilila , amakhala wotetezeka . ” Conco tingathe kuona kuti mapemphelo amene Kathy anali kupeleka anamuthandiza kukhala pa ubwenzi wolimba ndi Yehova . Ndithudi , tili m’gulu lodalilika , lotetezeka , ndiponso limene silidzatha . Iye amalandila zimene tingakwanitse , ndipo amayamikila kwambili . — Aheb . Conco , pa zifukwa zimenezi , mabuku athu a m’zaka zino amagogomezela kwambili mfundo zimene tikuphunzilapo pa nkhani za m’Baibulo , m’malo mofotokoza zinthu zimene nkhanizo zimaimila . 5 : 6 , 7 ) Sitiyenela kukhala aulesi , ndi kuyembekezela kuti Yehova adzabweletsa cakudya ndi kuciika pa thebulo . N’cifukwa ciani kukumbukila zifukwa zimene timagwilila nchito yolalikila n’kofunika ? NGATI munadwalapo mwakayakaya , mwina munadzifunsapo kuti , ‘ Mwati ine ndidzacila ? ’ Mu January 1981 , pamene Mairambubu anali m’basi paulendo wopita ku msika , anamvetsela zokamba za mzimayi uja amene nachula kuciyambi . Kodi nkhani imeneyi ndi yacisinsi ? ( Yes . 48 : 17 ) Tiyenela kudzicepetsa ndi kuvomeleza mfundo ya m’Mau a Mulungu yakuti : “ Munthu wocokela kufumbi alibe ulamulilo wowongolela njila ya moyo wake . 15 , 16 . ( a ) N’cifukwa ciani timamvetsetsa mmene ena amamvelela ? Anthu ena amene timaphunzila nao Baibulo , samakhulupilila kuti Yehova ali ndi gulu limodzi cabe padziko lapansi . 25 : 21 ) Malinga ndi Cilamulo ca Mose , munthu anayenela kuthandiza mdani wake ngati nyama yake yalemedwa ndi katundu . ( Eks . Cikhulupililo cinatilimbikitsa kudzipeleka kwa Yehova , komanso kukhala mabwenzi ake , zinthu zimene sizikanatheka popanda thandizo lake . — Aefeso 2 : 8 . Conco , makolo anga anapempha M’bale Atkinson kuti tsiku lililonse azibwela kunyumba kwathu kudzadya nase cakudya camadzulo , na kudzayankha mafunso ambili a m’Baibo amene tinali nawo . Baibulo limati : “ Iye anam’konda kwambili . ” — Genesis 24 : 67 ; 26 : 8 . ( Mat . Cinsinsi Namba 5 Kukambilana Kupambana misonkhano ina yonse ya anthu a Mulungu , Cikumbutso cimapeleka umboni wamphamvu kwambili wakuti Mboni za Yehova n’zogwilizana . Ena mwa io akhala akuzunzidwa , kuikidwa m’ndende , kapena kuphedwa kumene cifukwa cokhala okhulupilika kwa Yehova . BUNGWE LA AKULU : Dikishonale ina inakamba kuti mafaelo ofotokoza za Pontiyo Pilato ndi “ ambili ndipo amafotokoza zinthu zambili zokhudza iye kuposa za bwanamkubwa waciroma aliyense amene analamulilapo mu Yudeya . ” — The Anchor Bible Dictionary . Khalidwe loyamba limene Paulo anachula pa makhalidwe amene mzimu woyela umabala ni cikondi . Nchito yophiphilitsa yolekanitsa nsomba siikuimila ciweluzo comaliza cimene cidzacitika pa cisautso cacikulu . Motelo , tiyenela kupitilizabe kukambilana ndi Mulungu mwa kuphunzila Baibulo ndi kupemphela nthawi zonse . Pano tikamba , kudela limeneli kuli Mboni zambili . Yehova watiuzanso za makhalidwe ake . Khungu lake linali lofiilila ndipo anali ndi maso okongola . Kuti uthengawo ufalikile , anali kukopela zolembedwazo bwinobwino ndi manja . Samuel anasintha . Komanso ana obadwa kwa iwo amaonedwa “ oyela , ” ndipo ni ovomelezeka kwa Mulungu . Kodi kumeneku si kuweluzilatu anthu ? Yesu anakamba kuti sitiyenela kudela nkhawa za tsiku lotsatila , cifukwa tsiku lililonse lili ndi zodetsa nkhawa zake . Ngati mtima wathu umangokhala pa udindo kapena kuchuka , tidziŵe kuti tikubyala mbewu ya kudzimvela ndi mpikisano , ndipo cophukapo cake cidzakhala kugwilitsidwa mwala koŵaŵa . Nchito imeneyi imaphatikizapo nchito imene Yesu anagwila ali kumwamba ndi pamene anali padziko lapansi . ( Yoh . Ngati muona kuti ena amalalikila uthenga umenewu , kodi amafalitsa m’dela lanu cabe kapena “ padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse ” ? Onani nkhani yakuti “ Palibe Munthu Angatumikile Ambuye Aŵili ” ndi yakuti “ Limbani Mtima Yehova ndi Mthandizi Wanu ” mu Nsanja ya Mlonda ya April 1 , 2014 , mapeji 17 - 26 . Timakhala acimwemwe cifukwa cakuti Yehova amatitsogolela ndi kutithandiza kucita zinthu zambili zabwino . 20 : 1 - 3 ) Popeza kuti Satana ndi ziŵanda zake sadzakhalako , Ufumuwo mwamsanga udzathandiza anthu kupindula ndi dipo lansembe la Yesu ndipo udzacotsa mavuto onse amene timakumana nao cifukwa ca ucimo wa Adamu . Conco , m’malo mokamba kuti , “ n’zakhala na cimwemwe . . . ” tifunika kukamba kuti nili na cimwemwe . Iye anati : “ N’naona kuti pamene niseŵenzetsa mfundo za m’Baibo kutonthoza anthu amene nimaphunzila nawo Baibo , imakhalanso njila imene Yehova amanitonthozela na kunilimbikitsa . ” Ndiyeno , mlongoyu anayamba kuganizila za khalidwe lake . ( Aroma 12 : 3 ) Komanso , m’malo mocitila kaduka munthu amene akupatsidwa ulemu pa zimene anacita , tiyenela kukondwela naye limodzi ngakhale tiona kuti nafenso tinafunika kulandila ulemu wofananawo . Kenako , Felisa anandiuza zimene anaphunzila . Mofanana ndi acinyamata amene takambilanawa , mwina inunso munaleledwa ndi makolo amene amatumikila Yehova Mulungu . Nanga , kodi Rabeka adzamukonda mwamunayo ? Macenjezo onsewa ndi umboni wakuti Yehova amasamalila mwacikondi aliyense wa ife . N’cifukwa ciani kucita zimenezi n’kofunika ? 11 : 8 - 10 . Paladaiso wauzimu amene tili naye ndi cozizwitsa m’dziko loipali lomwe lilibe cikondi . Danieli anali munthu waluso kwambili moti anapatsidwa maudindo apamwamba . Izi zikanakhalanso ciyeso kwa iye . Yosimbidwa ndi Geoffrey Jackson Conco nditsikila kwa iwo kuti ndiwalanditse . ” Baibo imapeleka malangizo osapita mbali pankhani imeneyi . ( b ) Kodi Msamariya anam’thandiza bwanji munthu amene anavulidwa , kumenyedwa ndi kusiidwa ali pafupi kufa ? Ngati mwakhala mukutumikila Yehova kwa zaka zambili , mwina mwaona kuti pakhala kusintha mmene zofalitsa zathu zakhala zikufotozela zocitika zina za m’Baibulo . Pofuna kusintha - sintha nkhani zophunzila , io amagaŵana zigawo za anthu osiyana - siyana a m’Baibulo ndi kuziŵelenga monga banja . Akazi ena amene anali ophunzila a Yesu anali kutumikila iye ndi atumwi ake . Mu July 1940 , anakwanilitsa colinga cake atafika zaka 15 . Ndipo muzichula makolo anu m’pemphelo . Ŵelengani Mateyu 13 : 45 , 46 . Kale , zofalitsa zathu zinali kufotokoza kuti Satana ayenela kuti sanatenge Yesu mwacindunji kupita naye ku kacisi kukamuyesa . Timaŵelenga kuti Sara anali ‘ kuona ’ khalidwe loipa . Liu limeneli linali kumveka m’zaka za m’ma 1800 ku California , U.S.A . , munthu wogwila nchito ku migodi akapeza golide . Mulungu adzagwilitsila nchito Yesu kucotsapo zinthu zoipa zimene Satana wabweletsa . — Ŵelengani 1 Yohane 3 : 8 . 1,459 Anthu ena amene anali monga ana olowelela amayamikila Yehova cifukwa ca cifundo cake ndiponso mmene mpingo unawathandizila ndi kuwasonyeza cikondi . Kenako mphesazo zinapsa , ndipo wopelekela cikhoyo anazifinyila m’cikho ca Farao . Paulo analembela Timoteyo kuti : “ Iwe wayesetsa kutsatila ciphunzitso canga , moyo wanga , colinga canga , cikhulupililo canga , kuleza mtima kwanga , cikondi canga , ndi kupilila kwanga . ” ( 2 Tim . ( Pitani polemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ANTHU APABANJA NDIPONSO MAKOLO ) Mofanana ndi Mose , na ise tizikondwela ena akalandila udindo umene ifenso tikanakonda kuulandila ? Komanso , polangiza Akhristu aciheberi , Paulo anati : “ Limbitsani manja amene ali lende ndi mawondo olobodoka , ndipo pitilizani kuwongola njila zimene mapazi anu akuyendamo , kuti ciwalo cimene cavulala cisaguluke polumikizila , koma cicilitsidwe . ” ( Aheb . Nayenso Paulo analembapo za kufunika ndi ulemu wake wa zacikondi m’cikwati . Anafunika kusankha kaya kutengela zocita za anthu a m’nthawi yake , kapena kufuna - funa Yehova , Mulungu woona , amene anapanga kumwamba ndi dziko lapansi . Mofanana ndi zimenezi , anthu ochuka a ku Yudeya sanali kumulemekeza Yesu cifukwa anali wocokela ku Galileya . ( Yoh . 12 : 27 , 28 , 31 , 38 , 40 , 43 ) Mosakayikila , Yehova anakondwela ngako kumvela olambila ake akuimba nyimbo zom’tamanda mocokela pansi pa mtima . ( Aroma 14 : 8 ) Ndipo tikuyembekezela mwacidwi nthawi imene Yehova adzaukitsa mabwenzi ake onse okhulupilika amene anafa . ( Mat . ( Mateyu 22 : 23 , 29 ) Mtumwi Paulo anati : “ Ine ndili ndi ciyembekezo mwa Mulungu . . . kuti kudzakhala kuuka kwa olungama ndi osalungama omwe . ” — Machitidwe 24 : 15 . ( Yohane 13 : 34 , 35 ) Zimene ndinaphunzila zokhudza Yehova zinandicititsa kukhala ndi cifuno com’tumikila . Mtsogoleli wina wacipembedzo , Stephen Langton , amene anadzakhala Bishopu wamkulu ku Canterbury , ndi amene anagwila nchitoyi . Yosefe anali kapolo wa m’nthawi yakale kwambili , koma Blessing anali kapolo wa m’zaka za m’ma 2000 zino . 4 : 6 , 7 ) Koma Kaini sanamvele . 5 , 6 . ( a ) Kodi makolo aciisiraeli anali mboni za Yehova m’njila ziti ? Kodi dzikoli limalimbikitsa bwanji anthu kusalemekeza cikwati ? “ Pamene mkazi wanga anayamba kuphunzila Baibulo , ndinaona kuti wasintha kwakukulu . Cocitika Cosaiŵalika pa Utumiki Wanga wa Ufumu ( M . Izi zathandiza kuti akhalebe ogwilizana . Akuluwo anakambilana nkhaniyo ndipo anali kufuna kuti amishonalewo apitilize ndi utumiki wao . ( Danieli 12 : 4 , 8 - 10 ) Conco , Mulungu saulula tanthauzo la mauthenga ena a m’Baibo mpaka nthawi yake yoyenelela itakwana . Patapita nthawi , Mwana woyamba kubadwa wa Mulungu anasonyeza kukhulupilika ndi cikondi kwa Atate ake ndiponso kwa “ ana a anthu ” mwa ‘ kusiya zonse zimene anali nazo , ’ ndi kukhala wofanana ndi anthu . ( 2 ) Kodi odzozedwa okhulupilika akhala akugwilitsila nchito bwanji uphungu wa m’fanizo limeneli ? William anakamba kuti kutsatila malangizo amenewa kunatithandiza kukhala ololela , kulandila uphungu wa abale akumeneko , ndi kutsatila mmene amacitila zinthu kuti tipambane polalikila kudziko latsopano . “ Kudzela mwa kumvela kwa munthu mmodziyu [ Yesu ] , ambili adzakhala olungama . ” Ngakhale n’conco , nimaona kuti ngati ataniuza kuti nikatumikilenso kumeneko , ningafunikenso kuphunzitsidwa . Onse amuna ndi akazi anali ndi ciyambi cabwino . Tikacita zimenezi , “ Mulungu wa mtendele ” adzatipatsa mtendele wa mumtima . — Afilipi 4 : 8 , 9 . Muzipempha Yehova kuti akuthandizeni kukaniza maganizo oipa . Pambuyo pake , tinasamukila ku Colorado kukatumikila kosoŵa . Kumeneko anakwela bwato ndi kupita ku Makedoniya . Cilamulo ca Mose cinali kuvomeleza mwamuna kuleka mkazi wake ngati “ wam’peza ndi vuto linalake . ” 15 : 19 . Maurizio anati : “ Gianni anali kukamba nane moona mtima ndipo anali kucita bwino . Ana a Nowa anazindikila kufunika kocita cifunilo ca Yehova , ndipo anagwilizana ndi zocita za atate ao . Ndi malo otani amene akazi ali nao masiku ano pa nchito yolalikila uthenga wabwino ? Kodi kukonda Mulungu kumatilimbikitsa kucita ciani ? N’ciani cimene tidzacita ngati timaona kuti Ufumu wa Mulungu ni wofunika kwambili ? Sitiyenela kunyalanyaza nchito yoyeletsa pa Nyumba ya Ufumu . Abale na alongo ku Myanmar anatilandila na manja aŵili ! ” Colinga ca ulendowu cinali kukathandiza gulu lalikulu la abale a kumeneko kuti agwilizanenso ndi gulu la Mulungu . N’cifukwa ciani tinalamulidwa kukonda mnansi wathu ? Kuwonjezela apo , anthu ambili sanali kudziŵa kuŵelenga . Zikomo kwambili . ” Zinthu ngati zimenezi zingacititse kuti cikhale covuta kupitiliza kuonetsa cifundo kwa anthu amene timawalalikila . Mkaziyu anafikila Yesu m’njila yosaloleka na Cilamulo ca Mulungu . Kukumbukila mfundo imeneyi kumatithandiza kukhala na cikhulupililo mwa iye . Cifukwa copitilizabe kucitila umboni ndi kukhulupilila nsembe ya Kristu , a khamu lalikulu adzapulumuka “ cisautso cacikulu ” cimene cidzaononga dziko la Satana . — Yoh . Ngakhale kuti palibe Mboni ya Yehova imene inaphedwa , ambili anataikilidwa katundu wao wonse . Conco , m’kupita kwa nthawi , amayi ake anapempha mkulu wina mumpingo kuti akaonane naye m’ndendemo . Zotulukapo zake , Hans anayamba kuphunzila Baibo . Palibe ngakhale mau amodzi omwe sanakwanilitsidwe . ” Kodi cisautso cacikulu cidzayamba bwanji ? Nkhani ya Eliya ingakuthandizeni kuona ngati mukali m’cikhulupililo , ndi kuyamba kudziona moyenela . N’zoonekelatu kuti zimene Baibulo limanena zokhudza mapeto a dziko ndi nkhani yabwino . Panthawi ya nkhondo yaciŵili ya padziko lonse , panali Mboni za Yehova zosakwana 110,000 . Mfumu ya Isiraeli yacikalambile inalandila mwa mzimu woyela mapulani akamangidwe ka kacisiyo . 3 , 4 . ( a ) N’cifukwa ciani Akristu sayenela kupeputsa malamulo ndi mfundo za m’Baibulo ? 20 : 20 ) Pamene ndinali kutumikila ndi M’bale Gardner , ndinayamba kuikonda kwambili nchito yolalikila . Tiyenela kucita ciani kuti tiike maganizo pa zinthu za mzimu ? Mashini amenewo anali kusonkhanitsa zigawo za mapeji 32 za mabuku , zimene pambuyo pake zinali kusokewa na mashini osokela mabuku . Anthu amene timaphunzila nao Baibulo amaona kuti malo athu olambilila ndi aukhondo , ndipo timavala bwino . Ŵelengani Mateyu 28 : 19 , 20 . Cifukwa cakuti Mariya anali mbadwa ya Mfumu Davide kupitila mwa mwana wa Davide , Natani . ( Machitidwe 20 : 35 ) Ndipo cimwemwe cimene cimabwela cifukwa copatsa , cimakula kwambili ngati wolandila mphatsoyo waiona kukhala yamtengo wapatali . Lembali limati : “ Ndipo aliyense woitana pa dzina la Yehova adzapulumuka . ” Ngakhale zili conco , Yehova waika malangizo m’Mau ake okhudza kukwatiwa kokha mwa Ambuye . Nthawi zambili , Mulungu anali kumulimbikitsa kudzela mwa Akristu anzake . M’tauni ina ya kumigodi ku Australia , anthu 1,500 anapenyelela filimu imeneyi . 5 : 22 , 23 ; Aheb . N’ciani cimene tiyenela kucita kuti titeteze ubwenzi wathu wapadela na Yehova ? Ngakhale kuti anthu ena anamuona ngati wamantha , iye anaona kuti zimene anacitazo inali njila yabwino yoyankhila anthu osayamikila “ ngale ” za mtengo wapatali za coonadi ca m’Baibo . — Mateyu 7 : 6 . Cifukwa cosoŵa cakudya cauzimu na mayanjano olimbikitsa , n’nakhala wozilala . kudzakusonkhezelani bwanji kutengamo mbali mokwanila m’nchito yolalikila ? ( Gen . 37 : 28 ) Yehova anali kuona zonsezi . Komabe , pokamba za masiku ano Yesu anati : “ Uthenga wabwino uwu wa Ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” Nalonso chimo likakwanilitsidwa , limabweletsa imfa . ” Mwacitsanzo , iye anapita ku cikwati kumene anasandutsa madzi kukhala vinyo wabwino kwambili . Ndi motani mmene acinyamata angacitile zinthu mogwilizana ndi acikulile ? Baibo siikamba zambili zokhudza m’bale wathu wokondedwa Gayo . Nanga mungamuone bwanji mnzanu amene wakupatsani mphatsoyo ? Iye anati : “ M’malo mokhala pa mpando wa mkulu wa pakampani , tsopano nimakhala pa njinga ya olemala . Muziyelekezela m’maganizo mwanu kuti mukuona kapena kumva zimene muŵelenga . Zinali ngati kuti kulila kwao kunamveka ku Rama , dela limene linali kumpoto kwa Yerusalemu . — Mat . 18 : 14 , 15 ) Kuwonjezela apo , Hezekiya anakonzekela m’njila zosiyana - siyana kuti ateteze mzindawo kwa Asuri . 5 : 4 , 5 ) Conco , panthawi yoyenela , muyenela kukumbutsa mwana wanu mokoma mtima mfundo zimenezi . Pamene Davide anafika , Yehova anauza Samueli kuti : “ Ndi ameneyu ! ( 1 Sam . 15 : 3 , 9 , 12 ) Pamene mneneli Samueli anauza Sauli kuti Yehova sanakondwele ndi zocita zake , Sauli anapeleka zifukwa zodzikhululukila ndi kuchula mbali ya lamulo ya Yehova imene iye anamvela . Ndipo analoza cala ena pa zolakwa zake . ( 1 Sam . Samuel anaŵelenga nkhani ya acicepele imene anapeza pa webusaiti ya jw.org . Mwacionekele , ena anali osauka , koma zopeleka “ anali kuzigaŵa kwa aliyense malinga ndi zosoŵa zake . ” ( Mac . TIYELEKEZELE kuti mufuna kupita ku tauni inayake yakutali kukacita zina zake zofunika kwambili . Kodi ulamulilo wa Yehova umatipangitsa bwanji kumuyandikila ? Cikondico ndi lawi la Ya . ” — NYIMBO 8 : 6 . Tifunika kusinkhasinkha mmene zinthu zimenezi zimaonetsela kuti dipo ni mphatso yamtengo wapatali . — wp17.2 , mapeji 4 - 5 . Muziyamikila Mwai Wanu Wogwila Nchito ndi Yehova Tikatelo , m’pamene timakhala na umoyo waphindu . Kuti tikwanitse kucita zimenezi , tifunika kupitiliza kukulitsa cikondi cathu pa Yehova . Ni mavuto a bwanji amene munakumana nawo pamene munasamuka ? Nanga munalimbana nawo bwanji ? Mkazi wina dzina lake Raquel anati : “ Ndikaona mavuto aakulu amene anthu padziko lonse amakumana nao , zimandicititsa kuona kuti mavuto anga ndi ocepa kwambili cakuti ndimazengeleza kupempha Mulungu kuti andithandize . ” ( Ekisodo 21 : 23 ) Koma funso ndi lakuti , Kodi zikanatheka bwanji kuti moyo wangwilo umene Adamu anataya uomboledwe ? Mofanana ndi aphunzitsi a Baibulo a m’nthawi yakale , Mboni za Yehova masiku ano zikugwila nchito yophunzitsa anthu m’maiko 239 padziko lonse . Kuti asunge ciyelo ca mpingo , akulu anafunika kucotsa “ cofufumitsa ” pakati pawo . ( 1 Akor . ( Aroma 11 : 33 ) Kuti muwonjezele cidziŵitso canu , seŵenzetsani zida zofufuzila zimene zilipo m’cinenelo canu . Mumamva bwanji kuti muli ndi mwai wotengako mbali panchito monga alengezi a Ufumu ? Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse isanayambe , pa mipingo 84 imene inali ku France 32 , inali ya anthu okamba Cipolishi . Ena amafunitsitsa kufika pa misonkhano ya mpingo kapena ikulu - ikulu , koma thanzi lao limawalepheletsa kutelo . Kukamba zoona , nkhawa sizingatalikitse moyo wa munthu . Ndipo m’pomveka , cifukwa cinacokela kwa Atate ake , Yehova , amene ni wofunika ngako mu umoyo wake . Koma onse analephela . Kucitapo kanthu kwao mwamsanga kunawapulumutsa . Kusinkhasinkha zinthu za kuuzimu : Kumatanthauza kuganizila mozama za cilengedwe ca Mulungu , kapena zimene mwaŵelenga m’Baibulo ndi m’zofalitsa zathu . Lionetsanso kuti wopemphayu anali kudziŵa malamulo a m’Baibo , maka - maka a mu Levitiko na mu Deuteronomo , oletsa kucitila nkhanza anthu osauka . ” Kodi Rahabi anaonetsa bwanji kulimba mtima ? Iyai . Conco , tisamaope kuimba nyimbo zotamanda Yehova cifukwa coganiza kuti mau athu samveka bwino . Tiyenela kumaonetsa kuti tili na cikhulupililo m’malonjezo a Yehova . Banja lathu , ndipo Atate avala yunifomu ya usilikali N’zoonekelatu kuti Yehova afuna kuti anthu ocokela ‘ kudziko lililonse , fuko lililonse , ndi cinenelo ciliconse ’ apindule na Mau ake . “ Cifukwa ca kuwonjezeka kwa kusamvela malamulo , cikondi ca anthu ambili cidzazilala . ” — MAT . Cinyengo cingapangitse anthu ena kukhumudwa ndi kukwiya kwambili . Kumeneko , iye anali kukhala wotetezeka . Anthu amenewa anali kutsogoleledwa ndi Charles Taze Russell . Iwo anaphunzila nkhani yokhudza dipo la Kristu , ndipo mosataya nthawi anazindikila kufunika kwa dipo limenelo pokwanilitsa cifunilo ca Yehova . Ndimamvela bwanji ngati munthu wina wandikhumudwitsa ? Conco , ngati pali zinthu zina zake zovuta zimene mufunika kucita , muzikumbukila ciwombankhanga . Koma popeza kuti sakanatha kulimbana ndi Yehova , Mulungu wa Inoki , iwo anafuna kupha Inokiyo . Tuzidutswa twa golide nthawi zina tumapezeka m’mitsinje . Yesu sanali kufuna kucititsa manyazi mkaziyo kapena kum’dzudzula , koma anazindikila ululu wa matenda ake . Iye analitenga ndi kuliŵelenga . Pamene Sauli anayamba kulamulila , anali wofatsa ndi wodzicepetsa . Niyamikila kwambili Yehova kuti ni woleza mtima ndi wacifundo , ndipo amawamvetsa anthu amene amayesetsa kucita zimene Baibo imaphunzitsa . ( Aga . 5 : 26 ) Koma kudzicepetsa kumathandiza onse kuika pamodzi maluso awo kuti Mulungu atamandike , ndi kuti athandizane bwino lomwe . — 1 Akor . Kodi Asa anacita ciani pamene Aitiyopiya anaukila dziko la Yuda ? Funsani anthu ena kuti akuuzeni malemba ndi nkhani zimene zimawathandiza ndi kuwalimbikitsa . Iwo tsopano akufuna kuganiza paokha ndi kudzisankhila zocita . Tiyenelanso kuyesetsa kulimbana ndi maganizo olakwika kapena kuwathetselatu . Kodi tiyenela kucita ciani kuti titengele citsanzo ca Mariya ndi kuika maganizo athu pa kutumikila Yehova ? Antoine amene tsopano ali ndi zaka 90 , anati : “ Agogo anga a Joseph akamafotokoza Malemba Oyela , anali kuwalemekeza kwambili cifukwa ndi zimene atate ao anawaphunzitsa . Mtumiki amayang’ana kwa mbuye wake kuti am’patse cakudya na kum’teteza . Komanso amafuna kudziŵa zimene mbuye wakeyo afuna kuti iye acite , ndipo akadziŵa amacita zimenezo . “ Muzicelezana popanda kudandaula . ” — 1 PET . 25 Acicepele , Kodi Mumaika Zolinga Zauzimu Patsogolo ? Ni anthu ocepa cabe amene amaipeza . Pamenepo mudzapeza mfundo zothandiza pa nkhani zosiyana - siyana . Poceza , iye na mkazi wake nthawi zina anali kufunsana mafunso pa nkhani za m’Baibo . Ganizilani kuti mukuona Timoteyo akumvetsela mwachelu pamene Paulo ndi Baranaba akuuza Akristu amenewo kuti , ciyembekezo cao camtsogolo n’camtengo wapatali kuposa zimene akukumana nazo . 17 : 16 , 17 ) Ndiyeno , Mfumu ya Nkhondo idzaononga kothelatu dongosolo landale la Satana . Conco , Inoki anakhala mneneli woyamba amene uthenga wake unalembedwa m’Baibo . Tiyenelanso kukumbukila kuti popeza tonse tili ndi zofooka , ifenso nthawi zina tingakhumudwitse ena . Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Atakhala munthu , anadzicepetsa ndi kukhala womvela mpaka imfa . Koma cimene tidziŵa n’cakuti Yehova anafuna kuti anthu ake alalikile uthenga wabwino , ndipo Satana sanakwanitse kuwalepheletsa kucita zimenezo . 3 , 4 . ( a ) M’nthawi ya atumwi , ndi m’njila ziti zimene abale ndi alongo anatumikila Yehova ? ( b ) Nanga tingayandikile bwanji kwa Yehova ? 2 : 24 ) Izi zitanthauza kuti ngakhale mwamuna kapena mkazi , ‘ sayenela kulekanitsa cimene Mulungu anacimanga pamodzi . ’ Nthawi ina , iye anapempha Yehova kuti : “ Imvani mawu anga ocondelela pamene ndikufuulila inu kuti mundithandize . ” Ife coyamba tiyenela kukhala na cizoloŵezi cophunzila Baibulo . Dongosolo lonse la Satana , kutanthauza magulu a ndale , acipembedzo , ndi amalonda , onse adzatha nchito . Mosiyana na nyama , ise anthu tikhoza kuphunzila za Mlengi wathu na kum’tumikila mokhulupilika , ndipo kucita izi kumatipatsa cimwemwe . Anadziŵa kuti zimene Paulo anawalembela zinali zoona . Komanso , anthu amalemekeza kwambili asayansi , ndipo zimenezi zacititsa kuti asamalemekeze Mlengi . Mumtima mwanga ndinati , ‘ Uyu ndi mkazi wauzimu . ’ Ena amafunsa zimene angacite kuti acite bwino utumiki wawo pa Beteli . Tiphunzilapo ciani pa zimene Mose anacita cifukwa ca zolakwa za ena ? Ndipo anthu ena ambili ananenanso mau ofananawo . Kuwonjezela apo , Baibo siikamba kuti Yesu kapena munthu wina aliyense anali kukondwelela Khrisimasi . Paulo analembela abale a ku Korinto kuti : “ Ndikukutumizilani Timoteyo , popeza iye ndi mwana wanga wokondedwa ndi wokhulupilika mwa Ambuye . ( Lev . 19 : 18 ) Cikondi cimaticititsa kuti tizikondwela ndi coonadi , koma sicimatilole ‘ kukondwela ndi zosalungama , ’ ngakhale pamene mdani wathu akuvutitsidwa . — Ŵelengani Miyambo 24 : 17 , 18 . Jairo anali kukondwela kwambili ndi nkhani ya anthu opita ku ubatizo . Koma onani kusiyana pakati pa mmene Yehova amacitila zinthu na mmene Mdyelekezi amacitila . TSAMBA 19 • NYIMBO : 81 , 134 Athandizeni kukhala omasuka . — Mat . Iye analolela kugwilitsila nchito magazi a Mwana wake kuti tidzakhale na moyo wosatha . ( Yoh . Anationetsa buku lakuti Coonadi Cimene Cimatsogolela ku Moyo Wamuyaya . Komabe ine ndikukuuzani kuti : Usalimbane ndi munthu woipa , koma wina akakumenya mbama patsaya la kumanja , umutembenuzilenso linalo . ” Monga atsogoleli a anthu a Yehova , Mose ndi Aroni anali na udindo waukulu wopeleka citsanzo cabwino kwa anthuwo . ( Sal . 1 : 1 - 3 ) Amapeleka citsogozo pa nthawi imene tikucifuna . Ena amasankha kukhala ndi makolo ao kapena kukhala kufupi ndi kumene amakhala . Mkristu wozindikila amasankha zinthu zimene zingalimbitse ubwenzi wake ndi Mulungu Zikafika apa , mungafunike kucita khama kuti mupitilize kupeza mabwenzi atsopano . Kodi Yesu anali kutanthauza kuti abale ake ambili odzozedwa adzakhala oipa ndi aulesi ? ( b ) Kodi Aisiraeli anacita ciani m’malo modalila Yehova ? Iye anaseluka m’basi kuti aone zimene zinali kucitika . Ataseluka , anapeza mnyamata wacichainizi akukamba Cisipanishi movutikila pofotokozela msilikali wolondela malile a dziko za vuto lake . Koma pa nthawiyo , sin’nali kuseŵenza cakuti zinali zonivuta kupeza ndalama zoyendela . Koma m’kupita kwa nthawi , mungagule mukaona kuti angathe kupalasa . Sanalinso kugonjelanso ku zilako - lako zawo zaucimo . Lonjezo lokondweletsa limeneli linapelekedwa kwa mtumwi wokhulupilika Yohane , amene anauzidwa kuti : “ Lemba , pakuti mau awa ndi odalilika ndi oona . ” ( Chiv . Pa Agalatiya 6 : 5 pamati : “ Aliyense ayenela kunyamula katundu wake . ” Marilyn anaona kuti ngakhale kuti iye ndi mwamuna wake sanacite cigololo , io analephela kutsatila malangizo a m’Baibulo okhudza cikondi ndi kupatsana mangawa a m’cikwati cifukwa cosakhala pamodzi . Imakambanso kuti inauzilidwa na Mlengi wathu . Ungatithandizenso kusankha zinthu mwanzelu . M’kupita kwa nthawi , ukapolo unapita patsogolo kwambili . Zoonadi , njila imodzi imene timaonetsela kuunika kwathu , ndi mwa kulalikila uthenga wabwino na kupanga ophunzila . ( Mat . Na colinga cabwino copanda dyela . Iye amati : “ Usacite mantha , pakuti ndili nawe . 8 : 28 . Yobu sanali Mwiisiraeli . Zinthu zimenezi sizingathandize Akristu kukhulupilila Yehova ndi malonjezo ake . Mwacionekele , iye anali ndi makhalidwe a kuuzimu amene akanam’thandiza kulela mwana wake wangwilo kuti akule . Atakhala wothaŵa - thaŵa kwa zaka zambili , Davide anakhazikika bwino m’nyumba yacifumu . Atafika ku malowo , anaona zithunzithunzi za zida zoopsa za nkhondo ndi za akazi ovala zovala zoonetsa thupi . Ndi umboni uti umene uonetsa kuti Yehova akuthandiza anthu ake masiku ano ? Iwo amafuna kukuthandizani kuti mukalandile mphoto ya moyo . Zili conco cifukwa cakuti m’masana a tsiku lotsatila , Yesu anaphedwa ndipo otsatila ake anabalalika . ( Yoh . Iwo anali kukaonetsa koini ikulu yasiliva , ndi ingo’ono ya golide imene inali yamphamvu kuŵilikiza kaŵili ndi ndalama ya siliva . ( b ) Kodi anthu adzacita ciani cifukwa ca zizindikilo zimene zidzakhala kumwamba ? Amadziŵa zimene timacita tikakwiya . Iye aganizila kuti ngakhale cilengedwe cili ndi ciyambi , ‘ nanga Mulungu anacokela kuti ? ’ A nkhosa zina , amene ali ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo wosatha padziko lapansi , adzasangalala nao pa cikwati ca Mwanawankhosa cimene cidzacitikila kumwamba . Kunena zoona , ine nifuna kukhala monga iwe . 25 Musalole Ciliconse Kukumanitsani Mphoto Nthawi zina ndimapumula ndili cogona uku ndikuŵelenga kapena kumvetsela nyimbo . ( Yoh . 11 : 25 ) Lonjezo limeneli lidzakwanilitsidwa . Koma mkazi wanga sanali kufuna Mboni za Yehova . Mulungu anauza Mose kuti : “ Ndikudziŵa bwino zoŵaŵa zawo . Koma mwamsanga mngelo uja anakankha mkaziyo na kum’bwezela m’ciwiyaco . Pamene nkhaniyi inafika pacimake , M’bale Rutherford anafunsa kuti , “ Kodi mukhulupilila kuti Mfumu yaulemelelo yayamba kulamulila ? ” Sitingafune kuti ena atiganizile kukhala anthu amwano kapena osaganizila ena . Motelo odzozedwa akalibe kutengedwa kupita kumwamba , coyamba ‘ adzasandulika , m’kamphindi , m’kuphethila kwa diso , pa kulila kwa lipenga lomaliza . ’ Iye anali mkazi wolimba mtima ndiponso wacikhulupililo . 1 : 8 ) Koma kusintha kumene kumacitika cifukwa ca uthengawu nthawi zina sikumaonekela , ndipo zotsatila zina za nchito yolalikila sizionekela nthawi yomweyo . Ndiyeno , tingalembe ciŵelengelo ca maola amene tathela wiki imodzi - modziyo pocita zosangulutsa monga zamaseŵela , kuonelela TV , kucita maseŵela a pakompyuta , ndi zosangulutsa zina zimene timakonda . 7 : 39 ) Izi zitanthauza kuti Mkristu wosakwatiwa ayenela kupewa kuyamba cisumbali ndi munthu amene si Mboni ya Yehova yobatizidwa . Ngakhale kuti Yehova analonjeza Davide kuti adzapitiliza kum’dalitsa , anamuuza kuti mwana wake , Solomo , ndiye adzamanga kacisi . Vesi 29 imaonjezelanso kuti , “ Olungama . . . adzakhala mmenemo kwamuyaya . ” Mbali yaciŵili imene imacititsa Baibulo kukhala losavuta kumvetsetsa ndi nkhani zake . Pamene ciŵelengelo ca apainiya cinali kuwonjezeka mofulumila , abale audindo anapanga makonzedwe a mmene angathandizile gulu la apainiyawo . Bwanji osakhala na colinga cakuti nthawi zonse , misonkhano isanayambe kapena ikatha , muzikambako na wacicepele mmodzi , pofuna kuonetsa kuti mumamuganizila ? Iye anati : “ Abale ngati sitigwilizana nao tsopano , mwina sitidzakhalanso ndi mwai wina . ” Amacita zimenezo kupitilila m’nchito yopanga ophunzila . Nikali kusangalala ndi utumiki wa pa Beteli . Buku lina lokamba pa zipembedzo linanena kuti nchito yolalikila ya Mboni za Yehova “ ndi yosiyana kwambili ndi zipembedzo zina . ” ( Aroma 10 : 17 ) Kodi Nowa anamva kwa ndani za Yehova ? ( Ŵelengani Yesaya 60 : 22 . ) Pamene Yesu anapeleka fanizo la nkhosa ndi mbuzi , anali kukamba zinthu zimene zidzacitika panthawi ya mapeto . NYIMBO : 113 , 114 Ndithudi , ngati alendo ndi abale a ku malo osoŵa acitila zinthu pamodzi , onse amakhala ndi ubwenzi wolimba mu mpingo . Nawonso anali opanda ungwilo , ndipo anakumana na mavuto ambili ofanana ndi amene ise timakumana nawo . ( Chiv . 5 : 9 , 10 ; 14 : 1 ) Yesu ndi olamulila anzake , amene onse amapanga Ufumu wa Mulungu , adzathandiza mtundu wa anthu kupindula ndi dipo kwa zaka zoposa cikwi . Ine ndi anzanga atatu tinabatizikila m’cibafa cija pa November 12 , 1949 . Kodi lemba la 1 Akorinto 13 : 7 , 8 , litiphunzitsa ciani pankhani ya cikondi ? Uwu ni uthenga umene nakhala nikulalikila kwa zaka 25 . ” Mwina munafeledwa mnzanu wa m’cikwati , amayi , atate , kapena ambuye anu . Mwinanso muli na cisoni cifukwa munataikilidwa mwana . Pokhala wacikalambile , iye anauza Davide kuti sanafune kukakhala mtolo kwa mfumu . Onani mfundo zitatu za m’Baibo zimene anthu ambili samvetsetsa . Conco , tinakondana kwambili . ” — Karen , Northern Ireland . ( 2 Akorinto 7 : 1 ) Anthu amaipitsa matupi awo ngati amatafuna kapena kupepa fwaka , komanso ngati akumwa moŵa mwaucidakwa na kuseŵenzetsa amkola bongo . Kukamba zoona , ndinasangalala kwambili kupezekapo . ” — George , wa zaka 58 . ( Luka 11 : 13 ) Yehova analonjeza kuti ngati timupempha kuti atithandize , “ mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima [ yathu ] ndi maganizo [ athu ] mwa Khristu Yesu . ” ( a ) Malinga ndi Mateyu 6 : 19 - 21 , n’cifukwa ciani tiyenela kudziunjikila cuma cosatha ? Apa “ tsiku laciweluzo ndi cionongeko ” limene likubwela , aliyelekezela ndi kuonongeka kwa dziko m’masiku a Nowa . Ganizilani zimene zinacitika mu 1973 . Malinga n’kunena kwa anthu osakhulupilila Baibo , kodi zingakhale zoona kuti kuseŵenzetsa malangizo a m’buku lakale limeneli kungakhale monga kuseŵenzetsa kabuku kacikale - kale ka malangizo pa za sayansi kapena a kompyuta ? ( Agalatiya 2 : 4 , 5 ; 1 Yohane 2 : 19 ) Ndiponso odzozedwa ena angakhale osakhulupilika m’kupita kwa nthawi . Pa nthawiyi , amayi anabwela kudzakhala ku London . N’cifukwa ciani kugwilitsila nchito dzina la Yehova kapena kukhala mbali ya mpingo sikokwanila ? Cacitatu , timayesetsa kuona zabwino mwa anthu , kuphatikizapo zizindikilo zoonetsa kuti angathe kukhala atumiki a Mulungu . 41 : 13 ; 49 : 15 . Amuna olimba mtima amene amadzipeleka kulandila maudindo ni dalitso mumpingo . ( 1 Tim . Nthawi zambili , amene anayamba upainiya asanaloŵe m’banja , amapitiliza kucita utumikiwu akaloŵa m’banja . — Aroma 16 : 3 , 4 . Katswili wina wa Baibulo dzina lake Bruce Metzger , anati : “ Kuyambila zaka za m’ma 500 C.E . , ” mawu amenewa anali “ kupezeka kwambili m’mipukutu ya Cilatini Cakale ndi Baibulo la Cilatini lochedwa Vulgate . ” Nyengo yogwila nchito imeneyi ikakwana , alongo a kufupi ndi famuyo anali kubwela kudzaseŵenza nafe , ndipo mlongo Etta anali kuwayang’anila . Kodi inuyo mukanakhala ndi mphamvu yopatsa anthu zinthu zofunikila pa umoyo , simukanacita zimenezo ? 14 , 15 . ( a ) Ena aonetsa motani kuti amayamikila mwai wao wogwila nchito ndi Yehova mosasamala kanthu ndi nchito imene apatsidwa ? Mungapite kwa m’bale kapena mlongo wanu ndi kukambilana naye mokoma mtima ndi modzicepetsa kuti muthetse nkhaniyo . Kucita izi kumakhalanso kothandiza kwa abale na alongo amene amacita ulaliki wa pa kasitandi . 13 Kupangitsa Cikwati Cacikhiristu Kukhala Cacimwemwe Patapita zaka zambili Hezekiya atamwalila , mtsikana wina wodzicepetsa dzina lake Mariya , anali paubwenzi wapadela ndi Yehova . Ena amaopa kutaikidwa ulamulilo , poganiza kuti acinyamata sangayendetse bwino zinthu . ( 1 Timoteyo 6 : 9 , 10 ) Kodi zopweteka kapena kuti zoŵaŵa zimenezi zingaphatikizepo ciani ? A Zulu : Pamene Yesu anali pa dziko lapansi , anaonetsa kuti nthawi zokwanila 7 zinali zisanathe . Komanso , kupatsa kuli na ubwino wake kwa ise , kusiyana n’kumangolandila zinthu kwa ena . “ Dipo lolipilidwa ndi Khristu Yesu ” limaonetsa ‘ kukoma mtima kwakukulu ’ kwa Mulungu . — Aroma 3 : 24 . Kodi akulu amene amapatula nthawi kuti aphunzitse ena tiyenela kuwaona bwanji ? Kodi cilango cingaphatikizepo bwanji kuphunzitsa na cibalo ? ( b ) Kodi anthu mwacibadwa amafuna ciani ? Koma si zokhazo , naonso ana aamuna a Naboti anaphedwa . Masiku ano , Akristu odzozedwa naonso amaika maganizo ao pa Ufumu wakumwamba wa Mulungu , ndi pa ciyembekezo cao codzakhala “ olandila coloŵa anzake a Kristu . ” Kodi tidzaonetsa kuti timakhulupilila Yehova mwa kum’pempha kuti atithandize kukhalabe okhulupilika ndi acimwemwe ? ( Afil . ( Ezek . 38 : 18 - 23 ) Ndiyeno Mulungu adzaononga anthu onse amene adzafuna kuononga anthu a Yehova . Conco , tiyeni tizilimbikitsa mtendele mwa kuyesetsa kuthetsa mikangano imene ingabuke pakati pathu . Iye anati : “ Nyumba yathu inaonongeka ndipo ambili a m’banja lathu anaphedwa ndi cimpemphoco . ” ( Mat . 5 : 3 ) Motelo , iye “ wacititsa khungu maganizo a anthu osakhulupilila , kuti asaone kuwala kwa uthenga wabwino waulemelelo wonena za Kristu , yemwe ali cifanizilo ca Mulungu . ” — 2 Akor . 26 : 8 - 10 ) Nkhani imeneyi ili ndi phunzilo lalikulu kwa ife . Ana sabadwa na nzelu zosiyanitsa cabwino na coipa . Amafunika kuphunzitsidwa ( Onani palagilafu 8 ) Kuyambila ali mwana , anali kusungulumwa kwambili ndi kudziona ngati wosafunika . Mitima yathu imakhudzika tikaona mmene Yehova amayankhila mapemphelo athu . — Aheb . Yehova anasankha Aroni kutumikila monga mkulu wa ansembe wa Isiraeli , ndipo ana ake anali kutumikila monga ansembe . Komanso cifukwa cakuti sitifuna kucita cimo , timam’pempha kuti asatilowetse m’mayeselo . — 1 Yoh . 3 : 4 , 6 . ( Mateyu 6 : 10 ) Ufumu wa Mulungu udzacotsa nkhawa zonse kwamuyaya . Timalimbikitsidwa kufunafuna anthu amene angakhuzidwe ndi nkhani inayake yopezeka m’magazini athu . Kuti titsanzile nzelu za Mulungu , tiyenela kuganizila mwakuya mavuto amene angabwele cifukwa ca zocita zathu . Ndipo io anali ofunitsitsa kuuzako ena coonadi cimeneci . Zonse ziŵili ndi zinenelo za anthu a ku America . Ndipo n’nali kum’condelela kuti anithandize kuti niyambe kukhala na maganizo abwino . N’ndani wa ise amene sangakonde kukhala ku mbali yake ? Koma ndi thandizo la Yehova , ndife okonzeka kupilila ndi kupitiliza kumukhulupilila . — Miyambo 3 : 5 , 6 . [ Mau okopa papeji 15 ] Mfundo za m’Baibulo zimaticinjiliza ku cipembedzo conyenga ndi zamalaulo zimene zimamanga anthu mu ukapolo . ( Sal . Tatyana Kufuna kudziŵa colinga ca moyo kunacititsa Alexei kuphunzila Baibo . Popeza tinalibe zofalitsa m’cinenelo cao , tinadzifunsa kuti : Kodi tidzagwilitsila nchito ciani pophunzila nao ? Sizingatheke kuimba mwamphamvu na mokweza ngati simutsegula pakamwa mokwanila . Ambili amene timakumana nawo ali na umoyo umene n’nali nawo poyamba , wocilikiza Cikomyunizimu na kukhulupilila kuti kulibe Mulungu . ( Ekisodo 23 : 14 - 17 ) Koma Yesu anakamba kuti zonsezi zidzatha , ndipo “ olambila oona ” adzalambila Mulungu “ motsogoleledwa ndi mzimu ndi coonadi . ” Tikayang’ana zinthu zimene analenga , timaphunzila kuti ndi wamphamvu ndiponso wanzelu . ( 1 Pet . 5 : 8 ) Motelo , m’nkhani ino tikambilana makhalidwe atatu a Satana amene akuonetsa kuti tifunika kusamala ndi mdani woopsa ameneyu wa Yehova ndi anthu Ake . Marilyn anazindikila kuti sangalele mwana wake mwa kugwilitsila nchito foni , makalata , kapena mwa kukamba naye pa intaneti mwa kugwilitsila nchito kompyuta ya kamela . Conco , tinanyamula katundu wathu yense na kuthaŵa potulukila ku khomo la kumbuyo kwa nyumbayo , ndipo sitinabwelelenso . * Ngakhale kuti anafunikila kusintha zinthu zina paumoyo , io amaona kuti kucita zimenezo kunali kwa phindu . Kudzimva wokhutila kwanithandiza kuti nizikonda nchito . Yehova amatipatsa mphamvu ya mzimu woyela kuti itilimbitse ndi kutithandiza kulimbana ndi mayeselo . Khalani ndi Cikhulupililo Ndipo Muzipanga Zosankha Mwanzelu , Mar . ( Miyambo 11 : 2 ) Pa lembali mau akuti “ anthu odzicepetsa , ” angaimile anthu acikulile amene amazindikila kuti sangakwanitse kucita zonse zimene anali kucita poyamba . Zimenezi zinaniŵaŵa kwambili ndipo n’nali kudziona ngati wacabe - cabe . 2 : 24 ) Yesu anali kudziŵa kuti kupumula n’kofunika . Komabe , anthu amenewo anafunika kuphunzitsidwa . Tinakatumikila limodzi ku Mexico mumpingo wa cinenelo ca manja , ndipo tinali kuthandiza anthu ogontha kuphunzila za Yehova . Zimene timasankha zingakhudzenso anthu ena . Ndithudi , ngati muonetsa ena cifundo , nanunso mudzapindula . Ngati kholo lokalamba limafunikila thandizo nthawi zonse , mwana wolisamalila angatope . Buku lina lofotokoza zinthu zakale limati : “ M’mabwinja a Yeriko anapezamo zinthu zambili zoumba . Dziŵani izi : Yesu Khiristu anali kulemekeza kwambili Malemba . Anali kuwaona kuti ni Mawu a Mulungu . ( Miy . 15 : 22 ) Kuti timvetsetse mosavuta nkhani zimenezi , tigwilitsila nchito liu lakuti “ mphunzitsi ” ponena za mkulu amene amaphunzitsa ena , ndi liu lakuti “ wophunzila ” ponena za m’bale amene akuphunzitsidwa . Baibulo limaonetsa kuti atumiki a Mulungu angakhalebe pamtendele ngakhale kuti pali kusamvana . N’cifukwa ciani n’nali kukonda Cikomyunizimu ? Asayansi samvetsetsa kuti ubongo wathu umakwanitsa bwanji kucita zinthu zodabwitsa zimenezi . Mofananamo , ena cingawatengele nthawi itali kuti ajaile mu mpingo watsopano poyelekezela na ena . Baibulo limakamba kuti pali “ nthawi yokhala cete . ” Panthawi ina , iye anasowa koma osati cifukwa cakuti anapita kukaseŵela ndi acinyamata anzake . Iye anali wofunitsitsa kutsatila malamulo athu , ndipo anavomeleza kuti analakwa . Ndimamva bwanji kukhala pakati pa anthu ocepa amene amadziŵika ndi Yehova padziko lapansi ? M’malomwake , linavulaza ‘ anthu amene analibe cidindo ca Mulungu pamphumi pao . ’ Yesaya anasangalala pamene anauzilidwa kulosela za ulamulilo wa Mfumu Mesiya , yemwe ndi Yesu Kristu kuti : “ Sadzaweluza potengela zimene wangoona ndi maso ake , kapena kudzudzula potengela zimene wangomva ndi makutu ake . Anakamba kuti n’nali “ mwana wosayenelela ” kukhala pa sukulupo . Umu munali m’mwezi wa May 1909 . Pa ulendowo , iye anatenga M’bale Huntsinger , amene anali kalembela . Anam’tenga n’colinga cakuti paulendo wautaliwo , azim’thandiza kulemba nkhani za mu Nsanja ya Mlonda . Kodi Ufumu wa Mulungu udzakwanilitsa ciani ? Nanga tingatsimikizile bwanji kuti Ufumu umenewo udzabwela ? Kodi mumamva bwanji kudziŵa kuti Yehova amakusamalilani inu panokha ? Mwacitsanzo , zaka zambili zapitazo , atumiki a Mulungu anali kugwilitsila nchito manyuzipepala polalikila uthenga wabwino . ( Aef . 6 : 11 ) Yesetsani “ kudziŵa bwino ” coonadi conse . ( Aef . Musaumilile maganizo akuti iye anacitila dala kukukhumudwitsani . ( Aroma 5 : 6 - 8 ) Dipo la nsembe ya Yesu linalipilidwa , osati cifukwa cakuti ndife oliyenelela iyai , koma cifukwa cakuti ndife okondedwa . Tikamaganizila mmene tapindulila na coonadi ca m’Baibo pa umoyo wathu , timayamba kucikonda kwambili . Ndipo n’napanga matyuni kuti niziyimba nyimbo za Masalimo . Cifukwa anali kukamba ndi Aisiraeli amene anali kale mboni za Yehova . Malipoti aonetsa kuti anthu opitilila 100 miliyoni afa pankhondo kucokela 1914 . ( Onani ndime 6 ) Mng’ono wanga Lauri anali kukhala ku France , ndipo Ramoni anali kukhala ku Spain . Ndiyeno iwo anamuyankha kuti : “ Kodi iweyo ndithu ukuganiza kuti ungadzakhale mfumu yathu ? ” Kwa ena , nchito kapena udindo ni cizindikilo ca ulemelelo wa munthu . Tiyelekezelenso kuti mpainiya wacicepele amene akukhala pakhomo pa makolo ake wapatsa makolowo ndalama zocepa kuti agulile zinthu zina zofunikila pa nyumba . 11 : 41 , 42 ; Sal . Popeza pali zambili zimene akulu amapenda pofuna kutsimikizila kuti munthu ni woyenelela kubatizika , sizicitika - citika kuti ubatizo wa munthu ukhale wosayenelela . Cifukwa cakuti iwo anali na udindo wothandiza kuti mtundu wa Aisiraeli ukhale woyela . Tikamalalikila ndi kupanga ophunzila , timadziŵa bwino makhalidwe apamwamba a Atate wathu wakumwamba . M’buku la Mateyu caputala 10 , muli malangizo amene Yesu anapatsa atumwi ake 12 . Yasmine anakamba kuti : “ N’napitiliza kupemphela kwa Yehova , ndipo anayankha mapemphelo anga . Nanga n’cifukwa ciani anapempha Mulungu kuti asam’patse cuma ? ( 1 Akor . 2 : 14 - 16 ; 3 : 1 - 3 ) Popeza akulu amakhala na maganizo a Khristu , nthawi zambili amaona mwamsanga zizindikilo zakuti Mkhristu wayamba kukhala na maganizo akuthupi . N’napezanso thandizo ku cipatala , kuyamba kuseŵenzetsa bwino nthawi yanga , ndi kupatula nthawi yopumula na kucita maseŵela olimbitsa thupi . Ganizilani mmene Eliya anamvelela pamene Yehova anamuuza zimene mfumu ndi mfumukazi Yezebeli anacita . Mu 2013 , anthu oposa 11 miliyoni anaonetsa cidwi mwa kupezeka pa Cikumbutso ca imfa ya Yesu . 41 : 10 . NYIMBO : 38 , 31 Atafika paboda , asilikali anatulutsa Milan ndi onse a m’banja lake m’basimo cifukwa codana ndi mtundu wawo . Koma analola Mboni zinazo kupitiliza ulendo . ( Aheb . 6 : 12 - 15 ) Abulahamu anayembekezela kwa zaka zambili kuti Isaki abadwe , koma sanafooke , ndipo Yehova sanamugwilitse mwala . — Gen . Abale ndi alongo ambili apeza cimwemwe coculuka cifukwa cogwila nao nchito yomanga Nyumba za Ufumu . mmene Yehova amamvelela tikapezeka pa misonkhano . ( Gen . 3 : 5 , 6 ) Kucokela pamene Mdyelekezi anapatutsa Adamu ndi Hava pa kulambila koona , iye anapitilizabe kucititsa anthu kukhala ndi mtima wodzikonda . ( Chiv . 20 : 1 - 3 ) Ulamulilo wa Yesu wa Zaka 1,000 ukadzatha , Satana “ adzamasulidwa m’ndende yake ” kwa kanthawi kocepa kuti ayese kusoceletsa anthu angwilo komaliza . Baibo imati : “ Yesu atadziŵa kuti iwo akufuna kumugwila kuti amuveke ufumu , anacoka ndi kupitanso kuphili yekhayekha . ” N’zoona kuti panthawi ina Yesu anati : “ Samalani anthu inu kuti musanyoze mmodzi wa tianati [ ophunzila a Khristu ] , cifukwa ndikukutsimikizilani kuti angelo awo kumwamba amaona nkhope ya Atate wanga wakumwamba nthawi zonse . ” Ngakhale kuti ana ake aamuna anali otetezeka ndipo anali kutali ku Midiyani , iye anapeleka malangizo ku mabanja aciisiraeli amene ana ao aamuna anali pa ngozi . ( Eks . Kuwonjezela apo , Yakobo anavutika na zocita za apongozi ake acinyengo , amene mobweleza - bweleza anayesa kumudyela masuku pa mutu . Kodi ndinu wopanikizika maganizo cifukwa cakuti moyo wanu uli pangozi kapena mukukumana ndi mavuto aakulu ? Yesu anakamba kuti ophunzila ake ni abale na alongo cifukwa amaona Yehova kukhala Atate wawo wakumwamba . Cifukwa cakuti atumiki onse a Mulungu akhoza kumva mwanjila imeneyi , kaya ndi odzozedwa kapena ai . Iwo anafunikila kupilila kutentha kwa dzuŵa ndi nyengo yozizila . ( Akol . 1 : 15 - 17 ) Baibo imakamba kuti angelo amenewa amatumikila Mulungu mwacimwemwe monga “ atumiki ake . . . ocita cifunilo cake . ” M’masiku ano otsiliza , timakumana ndi zinthu zambili zimene zimayesa cikhulupililo cathu . Wofufuza golide angapeze tuzidutswa twa golide m’miyala ikulu - ikulu . Onse amene amamvela Mulungu ayenela kukhala olimba mtima cifukwa angatsutsidwe koopsa . Iwo afunika kuika maganizo ao “ pa zinthu zakumwamba , osati pa zinthu zapadziko . ” — Akol . Kodi timayesetsa kukhala monga dothi lofewa limene Yehova angaumbile cinthu camtengo wapatali ? Hutter sanalemele cifukwa ca nchito yake yomasulila , ndipo mwacionekele Mabaibo ake sanagulidwe kwambili . ( Mat . 24 : 46 , 47 , 50 , 51 ; 25 : 19 , 28 - 30 ) M’buku la Mateyu , Yesu anatsiliza kukamba cizindikilo ca mapeto a nthawi ino mwa kufotokoza fanizo la nkhosa ndi mbuzi . Iye anati : “ Mwana wa munthu akadzafika mu ulemelelo wake , limodzi ndi angelo ake , adzakhala pampando wake wacifumu waulemelelo . Mipukutu ya ku Nyanja Yakufa inapezeka m’mitsuko imene anaisungila m’mapanga a m’zipululu . Mungacite ciani kuti mupewe kutengela maganizo a dziko ? Zimenezi ndiye zofunika , ndipo musacite mantha kapena manyazi na mmene mau anu akutulukila . Kuonjezela apo , anthu analengewa mwa njila yakuti azikwanitsa kuganiza mozama , na kukwanitsa kusiyanitsa cabwino na coipa , ndiponso ali na cikhumbo cofuna kudziŵa Mulungu na kukhala naye pa ubwenzi . Koma alengezi ena a ku Poland anatsala ku France ndipo anapitiliza kulalikila mwakhama pamodzi ndi abale ndiponso alongo a ku France . Kodi munthu wauzimu tingam’dziŵe bwanji ? Nkhaniyi ifotokoza zinthu zinai zimene zingatithandize kupilila , ndiponso zitsanzo zitatu za anthu okhulupilika amene anapilila . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Kugwila nchito iliyonse [ mwakhama ] kumapindulitsa . ” — Miyambo 14 : 23 . Imene inadzachedwa kuti Utumiki Wathu wa Ufumu . Kapena ungauze bwanji m’bale wako kuti , ‘ Taima ndikucotse kacitsotso m’diso lako , ’ pamene iwe m’diso lako muli mtanda wa denga la nyumba ? Kodi Ameneyo sangakhale wamkulu kuposa Yesu ? Nthawi zambili tinali kucita zionetselo zosakondwa ndipo tinali kutseka sukulu nthawi iliyonse imene tafuna . Kodi cikhulupililo n’cofunika bwanji ? Timafunika kudziŵa nthawi yabwino yofikila anthu . Tingaŵelengenso Afilipi 2 : 9 , pamene mtumwi Paulo anafotokoza zimene Mulungu anacita pambuyo pakuti Yesu wafa ndi kuukitsidwa . Baibo imafotokoza zimenezi mophiphilitsa mwa kunena kuti cinjoka cinakokolola gawo limodzi mwa magawo atatu a nyenyezi zakumwamba . ( Gen . Monga Marita , na imwe mungakhale na cidalilo cakuti akufa adzauka ( Onani palagilafu 19 , 20 ) Mitima yawo inali phaphapha cifukwa ca mantha pamene anali kuthawa m’bwalo la nkhondo . Komabe mosiyana ndi mng’ono wanga amene anali kudzawasamalila cifukwa cowakonda , ine ndinali kudzawasamalila cifukwa ca udindo . Yehova ndiye Mpatsi wa Moyo ndipo mwacikondi amapeleka zosowa kwa olambila onse oona . Anam’cititsa kuganizila zimene Yehova anakamba m’munda wa Edeni kuti mbeu ya munthu idzawononga Satana . “ Khalani olimba m’cikhulupililo ndipo mulimbane naye [ Satana ] . ” — 1 PET . Iye anati : “ Ndikuona kuti ndinacita bwino kwambili kubatizidwa . Iye anatitsegulila khomo , titelo kukamba kwake , n’colinga cakuti tikhale mbali ya banja la Mulungu . Acinyamata ambili amene analeledwa ndi makolo acikristu angalephele kuona kusiyana pakati pa paladaiso wa kuuzimu ndi dziko lamdima la Satana . Uwe anakamba kuti nayenso anafunika kutsatila citsanzo ca Davide . Pa ulendo wake woyamba , iye anayambila kucezela dziko la Ireland . Umu munali mu July , 1891 . Kodi mwaona kuti pamenepa akugogomeza mfundo yakuti aliyense ayenela kucita zimene mnzake amafuna ? Ngati mufuna kudziŵa zambili za mmene mungapindulile ndi makonzedwe amenewa , funsani wa Mboni za Yehova aliyense . Ngati tikhalabe ku mbali ya Yehova , kodi iye angatithandize bwanji ‘ kugonjetsa ’ zilakolako za ucimo ? Iye anacita ngozi m’mbali mwa mtsinje ndipo analemala n’kumayendela pa kanjinga ka olemala . M’mau ena , tinganene kuti iye anati : ‘ Palibe cimene cingakutetezeni kwa Asuri . Kudziŵa Mulungu . M’nkhani yaciŵili , tidzaona mmene citsanzo ca Yehova cingatithandizile kukhala na mtima wokhululukila ena , kulemekeza moyo , na kucita zinthu mwacilungamo . Koma popeza kuti panthawiyo Mabaibulo ambili anali m’Cilatini , kodi anthu wamba akanapindula bwanji na Malemba ? Perrine na Louis Kodi malonjezo a Mulungu ndikali kuwaona kuti adzakwanilitsidwadi monga mmene ndinali kuwaonela kale ? Cikhulupililo ca Timoteyo cinalimba , cakuti anabatizika na kukhala wophunzila wa Yesu . Pa zaka zonse zimene natumikila Yehova , naphunzila kuti kukhala okhulupilika kumafuna kupilila , ndipo mtendele umene Yehova amapeleka ni cuma cimene sitingaciyelekezele na cina ciliconse . ( Aroma 12 : 9 ) Mpake kuti Malaki atakamba za “ buku la cikumbutso , ” Yehova anakamba kuti padzakhala “ kusiyana pakati pa munthu wolungama ndi woipa ndiponso pakati pa munthu amene akutumikila Mulungu ndi amene sanatumikilepo Mulungu . ” — Mal . Vuto ndi lakuti anthu sadziŵa mmene angapezele mayankho m’Baibulo . YESU asanapite kumwamba , anauza ophunzila ake kuti : “ Mudzakhala mboni zanga mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ” Ngakhale n’telo , ndinapitiliza kupita ku chechi pa Sondo ndi kupemphela pemphelo la Korona tsiku lililonse . Paulo anapelekanso moni kwa Akhristu ena a m’nthawi yake , amene masiku ano si odziŵika kweni - kweni . M’Baibo , tingapezemo zonse zofunikila zimene zingatiteteze ku mabodza a Satana . — 2 Tim . Yehova akaona cinthu cina cimene tifunika kuongolela , amaticenjeza ndi kutithandiza kuona zimene tingacite kuti tikhalebe naye paubwenzi Umenewu ndi utumiki wopatulika . Sin’naphunzilepo citundu cina , ndipo n’nali kuona kuti siningakwanitse . ( Mateyu 22 : 21 ) Timapeleka “ zinthu za Kaisara kwa Kaisara ” mwa kumvela malamulo a boma , kulemekeza akuluakulu a boma , ndi kupeleka msonkho . Nayenso Börje wa ku Sweden wa zaka 85 anati : “ Ndimayesetsa kukhala pamodzi ndi acinyamata . Masomphenya Oonetsa Amene Ali Kumwamba , Na . Kodi Irene anadalitsidwa bwanji cifukwa cofunitsitsa kuuzako ena uthenga wabwino ? Ndiponso Farao analamula kuti ana onse aamuna Aciheberi ayenela kuphedwa akangobadwa . ( Eks . Komabe , anali na cidalilo cakuti ophunzila ake adzalimba mtima ndi kukhalabe okhulupilika olo atakumana ndi citsutso ca m’banja . Muzimulembelako ka uthenga ka cikondi mnzanu wa m’cikwati * Komabe , tiyeni tikambilane mbali yomaliza ya fanizo la Yesu , imene ikukhudza kwambili nthawi inayake yapadela . Nanga n’ciani cina cimene tingacite pocilikiza nchito yolalikila Ufumu ? Mungapitenso pa webusaiti yathu ya , jw.org . Pa nthawi ina , Yesu anapempha Mateyu Levi , amene anali wokhometsa msonkho , kuti akhale wotsatila wake . Mwa kuphunzila kukonda Yehova ndi kudziŵa mmene iye amaonela fodya , inunso mungaleke kukoka . N’zovuta kukhulupilila . ( Yes . 25 : 7 ) Palibe munthu amene angapewe ucimo ndi imfa . Ndipo mwa mau amodzimodziwo , kumwamba kumene kulipo panopa limodzi ndi dziko lapansi , azisungila moto m’tsiku laciweluzo ndi cionongeko ca anthu osaopa Mulungu . ” — 2 Petulo 3 : 5 - 7 . Mwacitsanzo , kwa zaka 40 , Yehova anapatsa mtundu wa Isiraeli mana na madzi pamene anali m’cipululu . ( Eks . Ndipo ena amene anali na makhalidwe abwino , pambuyo pake analephela kupeza ciyanjo ca Mulungu . Mabanjawa limodzi ndi anchito ena odzipeleka , anapitiliza kuthandiza mipingo kupita patsogolo . Pokamba za dziko la Paradaiso , Mulungu anati : “ Dziko lapansi lidzadzaza ndi anthu odziŵa Yehova . ” ( Yes . Ngakhale pamene anatsala pang’ono kumwalila , Renee sanaleke kuika maganizo ake pa nkhani ya ulamulilo wa Yehova . 3 : 1 - 4 . Komanso cofunika kwambili makolo afunika kudzifunsa kuti , kodi kucita zimenezi n’kogwilizana na Malemba ? Kuganiza mofanana ndi Khristu kumakhudza kakambidwe kathu , zocita zathu kunchito kapena ku sukulu , ndiponso zosankha zimene timapanga tsiku lililonse . Pokhala Akristu oona , tifunika kupitiliza ‘ kulankhula molimba mtima cifukwa ca mphamvu ya Yehova . ’ N’zocititsa cidwi kuona kuti woumba , angaumbe cinthu cokongola ndiponso codula kwambili kucokela kudothi . Zaka zambili pambuyo pake , Yesu anaphunzitsanso mfundo yomweyi . — Luka 20 : 25 . ( Mac . 1 : 4 ; 2 : 46 ; 5 : 20 ) Mwa apa ndi apo , Paulo anali kupita ku Yerusalemu . Sitiyenela kunyalanyaza zofooka zathu kapena kupeza zifukwa zodzikhululukila nthawi zonse . Timacita kuphunzila khalidwe limeneli . Angelo ni amene anawononga mzinda wa Yerusalemu . Anandilola , ndipo anapitiliza kundipatsa malipilo amodzimodzi . Ganizilani mmene mudzasangalalila pogwila nchito yokonza dzikoli kukhala paradaiso pamodzi ndi anthu ena , ndipo anthu onse akukonda Yehova monga inuyo . Ena anali kuŵelenga poyela makalata awo m’machechi . Mulungu sanatipange kuti tiziganizila zinthu zoipa . Olo kuti Kaini na Solomo anali kudziona monga olambila Yehova , n’cifukwa ciani Yehova analeka kuwayanja ? Posafuna kukhala ndi malingalilo olakwika amenewo , omasulila analoledwa kumasulila liu lakuti “ soul ” mogwilizana ndi nkhani imene akumasulila . Kudziŵa kuti Mulungu amatiyang’ana , sikuyenela kuticititsa kuganiza kuti iye amafuna kuona zimene timalakwitsa monga mmene anthu ogwilitsila nchito makamela amacitila . Analimbikitsidwa ataŵelenga lemba la Mateyu 6 : 1 - 4 ( Ŵelengani . ) Akazi awo anayesa kuwakhazika mtima pansi , koma sizinaphule kanthu . ( a ) Kodi Yehova watilemekeza bwanji potipatsa ufulu wosankha ? Udzapita kukaukila anthu amene anasonkhanitsidwa pamodzi kucokela ku mitundu ina , amene akusonkhanitsa cuma ndi katundu , komanso amene akukhala pakatikati pa dziko lapansi . ’ ” ( Ezek . Conco onse pamodzi ndi iye anakwana anai . ” ( Yohane 1 : 47 ) Natanayeli amene anali kuchedwanso kuti Batolomeyo , anakhala mmodzi wa atumwi 12 a Yesu . — Luka 6 : 13 - 16 . Ine mwacibadwa nimacita manyazi kulalikila mwamwayi . Mtsikana wina amene anali atasiya Yehova kwa zaka 5 anati : “ Sindiziŵa kuti ndingafotokoze bwanji mmene ndinamvelela kuona abale ndi alongo akundisonyeza cikondi cimene Yesu anakamba . Nchito yathu yolela ana inaoneka kutha mwamsanga pamene iwo anakula na kucoka pakhomo . Conco , n’nali kucidziŵako Cizungu cakuti n’nakwanitsa kumasulila nkhaniyo na nkhani zina pa misonkhano ina . Cilamulo ca Mulungu cinapatsa Isiraeli wakale dongosolo la malamulo ozikidwa pa cilungamo ndi kusakondela . Ndipo buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni limene timaphunzitsila Baibulo , lamasulidwa m’zinenelo zoposa 250 . “ Kodi Ndingatani kuti Kulambila Mulungu Kuzinditsangalatsa ? ” — mutu 38 M’malomwake iye anayankha mwamsanga kuti : “ Malemba amati . ” 1 - 3 . ( a ) Kodi zinthu zinali bwanji pakati pa anthu a Yehova pamene mneneli Zekariya anayamba utumiki wake ? Jerome anati : “ Ndaona kuti ndikayamikila m’bale wacicepele pa zimene anacita bwino mu ulaliki kapena pa ndemanga yokonzedwa bwino imene anapeleka , iye amakhala ndi cidalilo . PAMENE tinakhala ophunzila a Kristu , tinayamba ulendo . Mungapelekenso citsanzo ca lesipi ( malangizo ophikila ) , kuti muthandize mwana wanu kukulitsa cikhulupililo mwa Mulungu . Makolo ena sangafune kukhala ndi ana ao . Iwo angafune kukhala paokha kuti asakhale mtolo kwa ana ao . “ KODI mwamuna wamphamvu angakhale waphindu kwa Mulungu ? Samalani mmene mukucitila cifukwa Yehova Mulungu wathu si wopanda cilungamo kapena watsankho ndipo salandila ciphuphu . ” 3 : 21 ) Zimene Malemba amakamba pa nkhani ya mavalidwe ndi kudzikonza , zimatithandiza kudziŵa bwino kuti Wolamulila wa cilengedwe conse ali na mfundo zabwino zimene afuna kuti olambila ake oona azitsatila . Ngati tifuna kuti Yehova atiyanje ndi kutidalitsa , tiyenela kucilikiza gulu lake ndi kutsatila kamvedwe katsopano ka mfundo za m’Malemba . Cotelo , tingakhale otsimikiza kuti sadzaleka kukonda atumiki ake okhulupilika , kuwaona kukhala ofunika , ndi kuwayamikila pa zimene amacita . — Eks . 46 : 8 , 9 ) Upandu : Ufumu wa Mulungu unayamba kale kuphunzitsa anthu mamiliyoni kuti azikondana na kukhulupililana . 1 , 2 . ( a ) Ni mavuto ati amene abale na alongo athu ena akumana nawo ? Izi ni zina mwa zocitika pamene anthu amapeleka mphatso . Panthawi ino , ciŵelengelo ca anthu padziko lapansi caculuka kwambili . ( Aroma 3 : 23 , 24 ; 6 : 23 ) Kodi tingacite ciani kuti tipindule ndi cikondi cacikulu cimeneci ? Iye amafuna kukhala ndi zinthu zambili zakuthupi . 13 : 1 ) Pamene mavuto a zandale akucititsa anthu kukhala osagwilizana komanso aciwawa , ise Akhristu takhalabe ogwilizana ndi amtendele . ( Mlaliki 3 : 4 ) Komabe , si zosangulutsa zonse zopindulitsa kapena zotsitsimula . 2 : 2 ; Aheb . 5 : 5 , 6 ) Cacitatu , Yesu anadzozedwa ndi mzimu woyela osati ndi mafuta , ndipo ufumu wake si wa padziko lapansi koma ndi wakumwamba . Anthu a ku maiko otentha akathaŵila ku maiko ozizila , angavutike na nyengo yozizila , ndipo sangadziŵe zovala zamphepo zoyenela kuvala . ( Luka 5 : 12 ) “ Pamene anaona Yesu , munthuyo anagwada n’kuwelama mpaka nkhope yake pansi ndi kum’pempha , kuti : ‘ Ambuye , ngati mukufuna , mukhoza kundiyeletsa . ’ ” CAKA COBADWA : 1964 Kodi Yosefe anadalitsidwa bwanji kaamba kokhala pa ubale na Yehova ? Ndife osangalala kuti khamu lalikulu likukula mwamsanga , ndipo timadziŵa kuti Yehova akulikulitsa . — 1 Akor . Anapitiliza kuti : “ Cikhulupililo sicili ngati coloŵa . Kodi atumiki a Yehova oyambilila anacita ciani kuti cikhulupililo cawo cikhalebe colimba ? Kodi Baibulo Limati Ciani pa Nkhani ya Ukwati wa Amuna Kapena Akazi Okhaokha ? Mwakutelo , anagwilizana ndi Satana kupandukila Mulungu . Nawonso Ababulo akale anacilikiza zakuti mzimu sukufa . Nanga n’ciani cidzakhalapo pambuyo pakuti zimenezi zawonongedwa ? Ngati mavuto anu sakutha , musataye mtima cifukwa Mulungu adzakulimbitsani na kukupatsani mphamvu kuti mupilile . Cifukwa caciŵili cinali kubuka kwa mlili wa matenda a Fuluwenza mu 1918 . Mkwatibwi ameneyu ndi ‘ woyela ndiponso wopanda cilema . ’ N’nasankha kulekelatu moŵa . Iye anati : “ Ndinadabwa kwambili ndi uthenga wa m’Baibulo . Tiyeni tiyelekeze nkhaniyi ndi munthu amene anabadwa wakhungu . Yehova amatitsogolela ndi kutilangiza cifukwa amatikonda . 8 , 9 . ( a ) N’ciani cinacititsa mnyamata wina kuti afike pocita ciwelewele ? Ndipo n’zimene apainiya ambili anacita . Atate anali kuona kuti abale a pa Beteli amenewa anali odzicepetsa kusiyana ndi azibusa a chechi amene anali atawakhumudwitsa kwambili m’mbuyomo . Anthu ambili sanali kuwadziŵa a Mboni za Yehova . Kodi mbili ya Aisiraeli itiphunzitsa mfundo yofunika iti pankhani yopanga zosankha ? Omasulila akhala akukumana ndi mavuto ena pomasulila Baibulo la Dziko Latsopano la Cingelezi . Mau amenewa anamulimbikitsa ngako . ( Maliko 13 : 10 ) Kukamba zoona , uthenga wabwino umaonetsa kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova . ( Mateyu 11 : 28 - 30 ) Anthu ambili anabwela kwa iye cifukwa anali munthu wotsitsimula . Kukhala m’gulu la Yehova ndi cinthu ca mtengo wapatali . ” Kodi iwo adzacita ciani ? Kodi mukukumana ndi zinthu zopanda cilungamo ? 13 , 14 . ( a ) Kodi nkhani zandale ndi zacipembedzo zinayambitsa bwanji ciwawa na kupanda cilungamo ? ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino cojambulidwa pa manja . ) N’citsimikizo camphamvu cotani nanga kucokela ku kacilembo kocepetsetsa kaciheberi ! Si covuta kumvetsetsa ndi kufotokoza nkhani za anthu enieni amenewo , ndiponso zimene timaphunzila kwa io . — Aroma 15 : 4 . Kodi Yesu anatanthauza kuti tizibweleza mau a m’pemphelo lacitsanzo nthawi iliyonse imene tikupemphela monga mmene amacitila Machechi Acikristu ? Ndayamba kale kulandila mphoto cifukwa coyesetsa kukumbukila cikondi canga coyamba pa Yehova . Yehova afuna kuti tizikhala oyela . ( 1 Pet . 3 : 7 ) Amuna ayenela kudziŵa kuti mangawa a mucikwati satanthauza kugonana cabe . Pamene nkhaniyi inali kukonzedwa kuti ifalitsidwe , M’bale Nsomba anamwalila ali ndi zaka 83 . Conco , ngakhale kuti Inoki anali na zaka 365 , anali kuonekabe wamphamvu cakuti akanapitiliza kukhala na moyo kwa zaka zina zambili . Mwacitsanzo , n’nakamba nkhani yoyamba ya anthu onse monga woyang’anila wadela pamtetete patsogolo pa shopu ya m’mudzimo . Pofuna kuthandiza ana awo mwauzimu , n’cifukwa ciani makolo amene anasamukila ku dziko lina ayenela kuganizila mosamala za citundu ? Muzikhulupilila Yehova Nthawi Zonse N’cifukwa ciani tiyenela kukhala osamala anthu ena akatipatsa malangizo okhudza thanzi ? Ndipo pakati pa Mbonizo , panali wacibale wake . Posapita nthawi , Graham anapatsidwa utumiki wopelekela maikolofoni pa misonkhano . Iye anayamikila ngako udindowu . 23 : 24 , 25 . ( Ŵelengani Yohane 11 : 33 - 36 . ) “ Mukadzaona zinthu zonsezi , mudzadziŵe kuti iye ali pafupi , ali pakhomo peni - peni . ” — MAT . 2 : 7 , 8 ) Mulungu anatumiza angelo kuti akapulumutse Loti . Iye anati , “ Popeza asodzi amakhala nthawi yocepa , tikawapeza timayamba kuphunzila nao Baibulo nthawi imeneyo . Pamene Yesu anamulola , Petulo anatuluka m’bwato ndi kuyamba kupita kwa iye . Kacisi wa Yehova na guwa lake la nsembe zinali zitawonongedwa , ndipo ansembe sanali kugwila nchito yawo mwadongosolo . Poona zimene zinacitikazo , iye analengeza coonadi ponena za Yehova Mulungu ndi Cilamulo Cake kuti : “ Mukadzaweluza dziko lapansi , anthu okhala panthaka ya dzikolo adzaphunzila cilungamo . ” — Yesaya 26 : 9 . Ena amakamba kuti Mulungu sanalenge anthu kuti azikhala padziko lapansi kwamuyaya . 7 N’nali kuseŵenzela kopulintila mabuku , ndipo n’naphunzila kugwilitsila nchito makina opulintila . Timadziŵa kuti kukhulupilila malonjezo a Mulungu kungatithandize kukhala olimba panthawi zovuta . ( Aefeso 6 : 4 ) Motelo , mufunika kuonetsetsa kuti mukuphunzitsa ana anu nthawi zonse . Kaya kukhalabe wokhulupilika kwa Yehova kapena kukhala ku mbali ya Satana . Pa ulendo wina , n’nadziŵana ndi mlongo Janet Dumond , mmishonale wa ku Thailand . 24 : 3 , 7 , 14 ; Luka 21 : 24 ) Conco , kucokela nthawiyo , “ zinthu zazikulu za Mulungu ” ziphatikizapo Yehova kuika Yesu monga Mfumu yolamulila anthu padziko . Kuphunzila kugwila nchito molimbika kuli monga kucita maseŵela olimbitsa thupi . Popeza ndife opanda ungwilo , nafenso tingacite zolakwa ngati zimene anacita mafumu anayi amene takambilana m’nkhani ino . Tsiku lina , Toñi amene amasamalila okalamba , anagogoda pakhomo ndipo mzimayi wa zaka za m’ma 50 anatsegula citseko . Ndiyeno dzifunseni kuti , ‘ Kodi n’kutheka kuti Mulungu akugwilitsila nchito anthu amenewa kuti andithandize ? ’ M’malomwake , nimayamba kukamba nkhani zina zolimbikitsa . Tiyeni tikambilane njila zisanu zofunika kuti banja likhale lolimba ndi lacimwemwe . Muthandizeni kukhalabe ndi makhalidwe abwino mwa kumupatsa nchito zina . Tate wina ku Germany amauzilatu banja lake zimene adzaphunzila milungu ingapo pasadakhale . Komabe , Davide mwana wa Jese sanali woyamba kubadwa . Alonso anali mu ukapolo wa mtundu wina . ( Yoh . 4 : 35 ) Inde , ngati mufuna kukatumikila kudela kumene minda ‘ ni yoyela ndipo ni yofunika kukolola , ’ yambani lomba kukonzekela kuti mudzakwanilitse colinga canu . Yehova amakufunilani zabwino , ndipo adzapeleka mphoto kwa amene amacita cifunilo cake . Yesu analamula ophunzila ake onse kulalikila . Kuonjezela pamenepa , palinso anthu ena amene amapindula ndi nchito imene timagwila . Magazini ya La Nación inakambanso kuti : “ Iwo anali paliponse mumzindawo , amuna ndi akazi , atavala zikwangwani zolengezela msonkhanowo . ” Monga Bwenzi lathu , Mulungu ni wokonzeka kutikhululukila na kutithandiza . — Salimo 86 : 5 . Iye anati : “ Ine Yehova ndine Mulungu wanu , amene ndimakuphunzitsani kuti zinthu zikuyendeleni bwino , amene ndimakucititsani kuti muyende m’njila imene muyenela kuyendamo . ” ( Yes . Koma n’cifukwa ciani iye sacita zimenezi ? Koma nikanakwanitsa kulamulila maganizo na zocita zanga . 6 : 11 , 27 ) Iye sanaumilile nga - nga - nga paudindo pofuna kuchuka ayi . Kodi tsopano muli ndi ana ? Tidzaonanso mmene makolo acikhiristu angapezele njila zokondweletsa zothandizila ana awo kukulitsa cikhulupililo mwa Mulungu ndi Mau ake . Cifukwa ca khama lao , Baibulo likupezeka m’zinenelo pafupifupi 2,700 kaya lathunthu kapena mbali yake . * Zikakhala conco , muyenela kukhulupilila kuti Atate wanu wakumwamba adzakuthandizani kumvela malangizo a m’Baibulo pankhani yokhudza wocotsedwa . Nanga mungacite bwanji zimenezi ? Mofananamo , tingakule mwauzimu pamene tiona zimene anthu acikulile kuuzimu amacita na kutengela citsanzo cawo . Koma tisaiŵale kuti “ Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima yathu ndipo amadziŵa zonse . ” Patapita zaka , Farao anamasula Yosefe m’ndende ndi kuika kapolo wodzicepetsayu kukhala wolamulila waciŵili mu Iguputo . Monga kholo lacikhristu , mumafuna kuti mwana wanu adziŵe malemba oyela , amene masiku ano amaphatikizapo Malemba Aciheberi na Malemba Acigiriki Acikhristu . Ndiyeno , dzifunseni kuti , ‘ Kodi nimacita zimene Yesu anaphunzitsa ? Koma palinso mbali ina ya Ufumu imene iyenela kukhazikitsidwa . Komanso tinali kuwauza mmene tinali kukondela utumiki wa umishonale . Salimo 102 ionetsa kuti ngakhale anthu amene ali m’cikhulupililo , angasautsike ndi kukhudzidwa kwambili ndi mavuto ao . Mabwenzi a Mulungu amakonda zimene iye amakonda na kudana na zimene amadana nazo . — Aroma 12 : 9 . M’fanizo la Yesu , mbewu imodzi ya tiligu inakula n’kubala mbewu zina ( kapena kuti zipatso ) zokwana 100 . Mmodzi mwa anthu amene anali kuseŵenza nawo , dzina lake Hans , anacita cidwi na khalidwe lake labwino . Wosimba ni Samuel F . Mu 1948 , Arthur anaweluzidwanso kuti akapike ndende miyezi itatu . ( Mat . 26 : 11 ) Kodi Yesu anali kutanthauza kuti nthawi zonse padziko lapansi padzakhala anthu osauka ? Iyai . Mlongoyu anati : “ Inali nthawi yovuta kwambili pa umoyo wanga . ” Nthawi zonse Ayuda anali kukumana m’masunagoge kapena pabwalo kuti alambile Mulungu . Monga Mlengi wathu wanzelu , amadziŵa zimene timafunikila ndiponso nthawi yabwino yotipatsa zimene tamupempha . Kuti mudziŵe mmene munthu angadzitetezele ngati wina afuna kumugwilila , onani nkhani yakuti “ Njira Zopeŵera Kugwiriridwa Chigololo , ” mu Galamukani ! ya March 8 , 1993 . Pambuyo pa milungu ingapo , ndinakhala wofalitsa wosabatizidwa . Patapita zaka zambili , Mfumu yoipa Ahabu , anali ndi mwai woona dzanja la Mulungu pa zocitika zosiyanasiyana . 5 : 1 - 3 ) Aja amene ndi zitsanzo zabwino mumpingo amapewa maganizo ndi zocita zosayenela . NYIMBO : 125 , 40 Munthu wakuthupi akakumana na ciyeso , amagonja mosavuta . ( Miy . Inde , Babulo Wamkulu anali ataŵafyanthilatu anthu mu ukapolo . 9 : 17 , 18 ; Agal . 1 : 14 ) Mosakayikila , mwadziŵa kuti mwamuna waciyuda amene tikukamba , ni uja amene anayamba kudziŵika kuti mtumwi Paulo . Tiyenelanso kupempha zosoŵa zathu za kuuzimu zimene n’zofunika kwambili . Anayambanso kudziyelekezela na coko , cimene munthu amatha kuciseŵenzetsa olo n’cophwanyika . KHALANI NDI MAGANIZO OYENELA : “ Masiku onse a munthu wosautsika amakhala oipa , koma munthu wamtima wosangalala amacita phwando nthawi zonse . ” “ Koma iye [ wophunzila wa Yesu Sitefano ] , pokhala wodzazidwa ndi mzimu woyela , anayang’anitsitsa kumwamba ndi kuona ulemelelo wa Mulungu ndi wa Yesu ataimilila kudzanja lamanja la Mulungu . Ndipo ananena kuti : ‘ Taonani ! Utumiki wathu , mgwilizano wathu wacikhristu , na kukhala kwathu maso mwauzimu , zonse zimapeleka ulemelelo kwa Yehova . Kodi iye anamvela bwanji kukhalanso m’nyumba yabwino , ndi kudya zakudya zabwino ? 3 : 16 ) Kodi pamenepa Paulo anali kutanthauza ciani ? ( Mwacitsanzo : Kodi nimasunga nthawi ? Monga mmene zinalili m’nthawi ya mtumwi Paulo , ambili masiku ano amapanga bajeti kapena kuika kandalama “ kenakake pambali ” kuti akaponye m’bokosi ya zopeleka za “ Nchito Yapadziko Lonse . ” N’zocititsa cidwi kuti m’kalata yake yaciŵili , iye anachula Paulo kuti “ m’bale wathu wokondedwa . ” Malinga ni buku lina lokamba za Ayuda , cioneka kuti banja la munthu wopha mnzake mwangozi linali kupita kukakhala naye ku mzinda wothaŵilako . Ndinabadwila mumzinda wa Baku , m’dziko la Azerbaijan , ndipo ndine wothela m’banja la ana aŵili . Koma akatswili ambili asayansi anali kukamba kuti ma IUD amalepheletsa mbeu ya mwamuna kukumana na dzila la mkazi kapena kulumikizana nalo . Nthawiyo , apainiya apadela anali kupeleka maola 150 pa mwezi . Conco , n’nakana mwayi umenewu . Kodi kukhala oceleza kungatithandize bwanji kuthetsa maganizo oipa amene tingakhale nawo okhudza anthu ena ? Ngati muganizila kuti ena sanakumvetsetseni kapena munacitilidwa mopanda cilungamo , musalole mkwiyo kusokoneza maganizo anu . Ngakhale kuti pa nthawiyo Timoteyo anali wacicepele , iye anali kuseŵenzetsa zimene anaphunzila . Anafuna kuti ndileke kuceza ndi mnyamata winawake amene anali kundikonda . Popeza kuti tili na Mau a Mulungu , omwe ni amphamvu kwambili , timafuna kuwaseŵenzetsa bwino . Mofananamo , khalidwe la anthu odziŵika ndi dzina la Mulungu limakhudza mmene anthu ena amaonela Yehova . Tingaonetse bwanji kuti timamvela malangizo a akulu ? Aisiraeli anali kutsatila Cilamulo ca Mose , ndipo cilamuloco cinali kuthandiza Ayuda onse okhulupilika pa nkhani ya makhalidwe . ( Luka 22 : 24 - 26 ) Mobweleza - bweleza , Petulo anacita zinthu zimene zinakhumudwitsa Yesu . Mosakayikila , iye anali kudziŵa bwino za adokowe amene anali kudutsa m’Dziko Lolonjezedwa . Iye anaphwanyaphwanya njoka yamkuwa imene Mose anapanga ” cifukwa masiku amenewo , anthu anali kuilambila . ( Aroma 10 : 4 ) Conco , funso lingakhale lakuti : Ndani amene anali ndi mwai wodzakhala ufumu wa ansembe ? A Daka : Inde ndikuvomeleza . Monga munthu wangwilo , iye anacita cifunilo ca Atate wake mokhulupilika . — Yoh . 1 : 1 - 3 , 14 . Fanizo la Yesu likugogomeza mfundo yakuti anamwali anzelu anali okonzeka za kubwela kwa mkwati kusiyana ndi anamwali opusa . Lembani zinthu zimene mufunikila . Anali kutifunsa za umoyo wathu ndi nchito imene tinali kugwila . Ndipo anali kutifunsanso ngati pali zovuta zilizonse . ( b ) Mofanana ndi Mose , kodi tiyenela kucita ciani ? Ponena za mau ake , motsimikiza iye anati : “ Sadzabwelela kwa ine popanda kukwanilitsa colinga cake , koma adzacitadi zimene ine ndikufuna ndipo adzakwanilitsadi zimene ndinawatumizila . ” — Yesaya 55 : 11 . Anthu ambili amapita ku tuakacisi topatulika cifukwa amakhulupilila kuti mapemphelo ao adzayankhidwa ngati apelekedwela pamalo amenewo . Nanga bwanji ngati wina akulephela kudzipeleka kwa Yehova , kodi zikutanthauza kuti iye adzakhala monga nsomba ‘ yosafunika ’ kwamuyaya ? Zikakhala conco , oweluza osati munthu wolakwilidwa anali kugwilitsila nchito mau akuti “ moyo kulipila moyo , diso kulipila diso , dzino kulipila dzino . . . ” Akulu amafuna kuti inu muzisangalala mu mpingo wanu watsopano , ndipo ni okonzeka kukuthandizani . Mwacionekele , mumasangalala kwambili mukamaganizila zimene mudzacita pamene Mulungu adzakwanilitsa colinga cake . Kodi Mulungu anamuyankha ? Koma inu mukhoza kupewa zimenezi . ( b ) Kodi mau a Yehova a pa Ezekieli 3 : 18 , 19 na pa caputa 18 : 23 amatilimbikitsa bwanji kupitiliza kulalikila ? Komanso , ophunzilawo anali kuonedwa kukhala osafunika m’dziko lao . ( Salimo 90 : 2 ) Mulungu amafuna kuti anthu azimufuna - funa ndi kudziŵa zeni - zeni ponena za iye . — Ŵelengani Machitidwe 17 : 24 - 27 . Pa Mateyu 6 : 33 , pali mau a Yesu olimbikitsa akuti Mulungu adzasamalila zosoŵa za atumiki ake okhulupilika amene amaika zinthu za Ufumu patsogolo . Baibulo limakamba kuti Yehova * Mulungu amadziŵa zonse . “ Wakumva pemphelo ” walonjeza atumiki ake kuti adzawapatsa ciliconse cimene akufuna kuti akhalebe okhulupilika kwa iye . ( Sal . Satagwanika m’maganizo ndi maudindo amene angapeze mtsogolo , kapena maudindo amene ena akupeza ayi . Iye anakwatila Yezebeli amene anapangitsa kuti kulambila Baala kufalikile m’dzikolo ndipo mfumu nayonso inayamba kulambila Baala . Pamene anali wacicepele , Solomo anali kuyang’ana kwa Yehova kuti am’patse malangizo . TSAMBA 19 • NYIMBO : 101 , 116 Koma boma la Nazi linali kudana naye . 14 : 13 ; 15 : 7 , 16 ; 16 : 23 . Cikhalidwe ca Agiriki citafala kwambili , anthu odzicha Akhristu , nawonso anatengela ciphunzitso cacikunja cimeneci . Acibale anga anali kunditsutsa m’njila zosiyanasiyana . ( 1 Akor . 3 : 9 ; 1 Pet . 1 : 15 ) Kulalikila uthenga wabwino kumathandiza kuti dzina loyela la Yehova liyeletsedwe . Yehova anateteza nchito imeneyi . Tinalibe wailesi , TV , ngakhale manyuzipepa . Conco , za nkhondo tinali kuzimvelako cabe kwa anthu ena . ( Mat . 5 : 43 - 45 ) Kaya anzathu ndi olungama kapena ndi osalungama , tiyenela kuwakonda . Kenneth Flodin ( Aefeso 4 : 23 ) Iwo aphunzila ‘ kukhala okhutila ndi zimene ali nazo ’ ndi kukhala ‘ oganizila zofuna za ena ’ m’malo mwa kukhala adyela ndi odzikonda . — Afilipi 2 : 4 ; 1 Timoteyo 6 : 6 . M’kilasi ku Sukulu ya Giliyadi , n’nali kukhala pafupi na M’bale Martin Poetzinger . 8 : 9 ; Yer . ( Yelekezelani na Ezekieli 28 : 17 . ) ( Sal . 13 : 5 , 6 ) Davide anakhulupilila kukoma mtima kosatha kwa Yehova . Ndikukhulupilila ndi mtima wanga wonse kuti limeneli linali yankho la mapemphelo anga . Palibe buku lina lacipembedzo limene limafanana ndi Baibulo pa mfundo zimene tafotokozazi . Ngakhale n’conco , macaputala ndi mavesi amatithandiza kupeza mau kapena mfundo inayake mosavuta , monga mmene tingaikile cizindikilo m’buku pankhani inayake imene timakonda . Kodi mabanja acikhristu angacite ciani kuti cikwati cawo cikhale colimba ? Pankhaniyi , mwina iye anagwilitsila nchito citsanzo ca mtengo wa maolivi . ( b ) Kodi Paulo analiseŵenzetsa bwanji liu lakuti “ thupi ” pa Aroma 8 : 4 - 13 ? Zinali zocititsa cidwi kuona kuti mfumu inalamulila zaka zambili conco m’zaka zathu zino . Njala na matenda obwela kaamba kopeleŵela kwa cakudya m’thupi , sizidzakhalakonso . Olo kuti lomba timakhala kutali ndi ana athu , ndise okondwa kuti nthawi zambili timakwanitsa kukamba nawo . ” Buku lina linakamba kuti Mfumu Nero akalandila mlandu , anali kuweluza mlanduyo limodzi ndi aphungu ake odziŵa bwino zinthu ndi anzelu . ( The Life and Epistles of Saint Paul ) Pamene tikonda kwambili Mulungu wathu , m’pamenenso cikhulupililo cathu cimalimba kwambili . “ Seŵelo la Eureka ” linafala ngakhale m’nyumba zoonetsela mafilimu . Mzimu woyela unalimbitsa amuna oimilako Mulungu . Nili na maphunzilo a Baibo atatu . Nthawi zina , tingalephele kuzindikila zinthu zofunika zimene tiyenela kupemphelela . Abale ndi alongo athu amatilimbikitsa pamisonkhano mwa kukamba nkhani , kupeleka mayankho , ndi kuimba nyimbo mocokela pansi pa mtima . Ngati tingayelekeze kuti tikuona Sara akuyang’ana ca kum’mawa mosakondwa , kuyewa zinthu zabwino za mumzinda umene anakulila , ndiye kuti sitim’dziŵa bwino mkazi woopa Mulungu ameneyu . Ngati ticita zimenezo , sitingakhale acimwemwe potumikila Yehova . Mwacitsanzo , pamene Aisiraeli anali kucita zopeleka zomangila cihema m’cipululu , ayenela kuti anapeleka zinthu zimene anatenga pocoka ku Iguputo . ( Eks . Anamuvula mwankhanza mkanjo wake wapadela , anamuguzila ku citsime ca matope ndi kumukankhilamo . 4 : 12 ) Kudzicepetsa kudzatithandiza kupewa kukhala “ wolungama mopitilila muyezo , ” ndi kunyoza anthu ena amene alibe maluso kapena maudindo amene tili nao . Mu 1934 , Bulletin inalengeza kuti pakufunika apainiya othandiza pamene inati : “ Kodi pangapezeke anthu 1,000 amene angalembetse podzafika nthawi ya Cikumbutso ? ” 18 : 26 ; 19 : 8 . Khalani citsanzo cabwino mwa kumulemekeza . Kuyamikila na kulimbikitsa ena mwa njila imeneyo kumakhala na zotulukapo zabwino ngako . ( 1 Atesalonika 5 : 14 , 15 ) Ngakhale pa nthawi ya cisautso cacikulu , tidzakhala olimba mtima , tili ndi cidalilo cakuti cipulumutso cathu cili pafupi . — Luka 21 : 25 - 28 . Tsiku limenelo , anthu 120 a mumpingo watsopano wacikristu anadzazidwa ndi mzimu woyela ndipo anayamba kulankhula zinenelo zosiyanasiyana kwa Ayuda ndi anthu otembenukila ku Ciyuda . Makolo acikhiristu angaonetse bwanji kuti ni okhulupilika kwa Mulungu ? Mkazi wapanyumba anali kusakaniza ufa ndi madzi , ndi kuyamba kukanda ufa umenewo . Inu Akhristu acicepele amene mumakana kucita zaciwelewele , timakunyadilani kwambili . Koma Marita anali wotangwanika . Tikamaŵelenga za ciwembu cimene Yezebeli anakonza , timanyansidwa ndi kuipa mtima kwake . mmene nchito yathu yafalikila padziko lonse ? Tingakonzekelenso kudzakhala ndi moyo m’dziko latsopano mwa kukhala oleza mtima pamene kamvedwe kathu ka coonadi kasintha . Ngakhale n’conco , munthu safunika kucita kudziŵa zonse kuti adzipeleke kwa Mulungu na kubatizika . Onani zimene imakamba pa mafunso ofunika kwambili otsatilawa . 20 : 10 ) Colinga ca Satana pogwilitsila nchito cizunzo ca mwacindunji kapena ca mwakabisila , ndi kufuna kuti atifooketse mwa kuuzimu kuti tileke kutumikila Mulungu . N’ciani cawathandiza kuti apambane ndi kukhalabe acimwemwe ? Muziuzako ena mfundo zimene mwapeza pophunzila Mau a Mulungu . Mwina munthuyo angayankhe kuti ngati io ndi mapasa . Koma kumbukilani kuti Yehova analenga dziko m’njila yakuti lizikhala ndi cakudya cokwanila , cimene ngakhale ana a makwangwala amalilila . Patapita miyezi yocepa kucokela pamene Yesu anakumana ndi munthu wakhate ku Galileya , iye anapita ku Yudeya kukalengeza uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . Nayenso Victoria wa zaka 23 anati : “ Ngati ukamba zoona na kuikila kumbuyo zimene umakhulupilila , ena angayambe kukuvutitsa . N’cifukwa ciani kukhala maso n’kofunika ngako ? Koma pa nkhani ya Azariya , Malemba ena amafotokoza mfundo zoonjezeleka . Ndunayo inayankha kuti : “ Ndingamvetse bwanji popanda wondimasulila ? ” ( Mac . Kuwonjezela pa Ayuda aciwawa amenewo , Ayuda ena ambili anali kuyembekezela mwacidwi kubwela kwa Mesiya . Kodi cikwati ca Mwanawankhosa cidzacitika liti ? Comvetsa cisoni kwambili n’cakuti “ Nkhondo Yaikulu ” imeneyo inabweletsa mavuto osaneneka . Yosefe atapita kukaonana ndi Pilato , anadabwa kuona kuti anamvela zimene anamupempha . Koma kodi Yehova amayankha bwanji mapemphelo athu ? Ngati sitingacitepo kanthu kuti tithetse vutolo , tingayambe kukhala wokhumudwa . — Ŵelengani 1 Petulo 3 : 8 , 9 . Acinyamata ena agwa m’ciyeso cofuna kulaŵa umoyo wa m’dzikoli . Kukada kapena ngati kukugwa mvula , akaidi sanali kuloledwa kuyendayenda . Anali kum’tumanso pa nkhani zina zacinsinsi . Pamene Abisalomu analanda ufumu Davide bambo ake , Aisiraeli ambili anakhala kumbali ya Abisalomu . Mosakayikila , pambuyo pobatizika , anapitiliza kuwonjezela cidziŵitso cake . Kodi anthu a Mulungu amaonetsa bwanji cikondi kwa anzao ? Cotelo kaya tikhale ndi moyo kapena tife , ndife a Yehova . ” ( 2 Akor . 11 : 29 ) Ponena za anthu a mumpingo , amene anayelekezela ndi ziwalo za thupi , Paulo anakamba kuti ziwalo zimene “ zimaoneka ngati zofooka ndizo zofunika . ” ( 1 Akor . Tonse timakumana ndi mavuto . Koma Yehova amatitonthoza . Kapena mungakumbukile kuti Yehova ni wacifundo ndipo amayembekezela kuti munthu alape ? Ndiyeno amanena kuti : “ Lelo tikupatsa kapepala aka kwa aliyense m’gawo muno . Mwacitsanzo , pamene Ezara anabwelela ku Yerusalemu , anatenga zinthu zimene mfumu ya Peresiya inapeleka monga copeleka . Katunduyo anaphatikizapo golide , siliva , na zinthu zina zimene mtengo wake masiku ano ungapose madola 100 miliyoni a ku America . Cilango cimatsogolela mwana monga mmene coongolela boti cimathandizila kuti iziyenda bwino Ganizilani zimene anakamba pa Ulaliki wake wa pa Phili wolembewa pa Mateyu 5 : 18 . Iye anati : “ Ndithu ndikukuuzani kuti kumwamba ndi dziko lapansi zingacoke mosavuta , kusiyana n’kuti kalemba kocepetsetsa kapena kacigawo kamodzi ka lemba kacoke m’Cilamulo zinthu zonse zisanacitike . ” Pamene Mose anali mwana , analeledwa ndi amai ake a Yokobedi , ndipo anakhala mtumiki wokhulupilika wa Yehova . ( Eks . 2 : 1 - 10 ; Aheb . Nanga Yehova amadalitsa bwanji zosankha zathu ngati timamuika patsogolo ? Ni cozizwitsa capadela citi cimene Eliya anacita ? Nanga cozizwitsaci cigwilizana bwanji na nkhani ya Marita ? 12 : 21 - 23 ) Ndithudi , palibe aliyense akanakamba kuti Herode anasankhidwa ndi Yehova kukhala mtsogoleli . 3 : 12 ) Iwo anagwila nchito ya pansi imeneyi ndi mtima wonse ngakhale kuti anali ana a kalonga . Baibo imene anamasulila inayamba kuchedwa kuti Baibo ya Cigiriki ya Septuagint . Timanyadila kudziŵika na dzina lake komanso kuliseŵenzetsa , podziŵa kuti kukonda Mulungu kumabweletsa madalitso oculuka kuposa kukonda ndalama na zinthu zina . — Yes . Posacedwapa , Mulungu adzaononga onse oipa . Kodi anacita ciani ? Conco , tikamapemphela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele timakhala kuti tikupempha kuti boma la Mulungu liloŵe m’malo mwa maboma a anthu . — Ŵelengani Danieli 7 : 13 , 14 ; Chivumbulutso 11 : 15 , 18 . Ngati mukukumana ndi ciyeso , fotokozelani akulu . ( b ) Nanga angacite ciani kuti asankhe mwanzelu ? Mfumuyo inauza anthu ake kuti : ‘ Taonani ! Ku Latin America , pafupifupi munthu mmodzi pa anthu atatu aliwonse , anakamba kuti anacitidwapo za ucifwamba . Zonse zimene tili nazo n’zocokela kwa iye . Timakumana ndi anthu “ odzimva , odzikweza , onyoza , . . . onenela anzawo zoipa , osadziletsa , [ ndi ] oopsa . ” ( 2 Tim . 4 : 13 ) Zitsanzo za anthu a m’nthawi ya Paulo ndi zamakono , zionetsa kuti kupemphela kumatithandiza kuti tikhalenso ndi mphamvu ndi kupilila . ( Yohane 11 : 17 , 21 ) Yesu anayankha kuti : “ Ine ndine kuuka ndi moyo . Anthu onse , maka - maka amene akunyansidwa ndi zinthu za m’dzikoli ndipo akufuna kudziŵa zambili za Mulungu amene timalambila , timawalandila ndi manja aŵili ku misonkhano yathu . Lekani nikuuzeni zina zokhudza umoyo wanga kuti mudziŵe cifukwa cake n’napezeka pa malo amenewa . Iye anati : “ Wina amaona tsiku lina ngati loposa linzake , koma wina amaona tsiku lina mofanana ndi masiku ena onse . Conco munthu aliyense akhale wotsimikiza ndi mtima wonse m’maganizo mwake . ” Tingakambe kuti dzikoli lili ngati munthu wopita kukanyongedwa ameneyu . Zimenezo zidzakhala zocititsa cidwi kwambili . 6 : 11 ) Koma sitingakwanitse kucita zimenezi mwa mphamvu zathu . Ndiye cifukwa cake , potengela citsanzo ca Akristu oyambilila , tizipemphela kwa Yehova kuti atipatse mzimu wake umene umapeleka “ mphamvu yoposa yacibadwa . ” — Ŵelengani 2 Akorinto 4 : 1 , 7 ; Luka 11 : 13 . Anthu ambili amene amaikidwa m’ndende amatulukamo bwino - bwino popanda kuwacotsela ulemu . ” Mlongo wina dzina lake Judy analemba kalata ku likulu lathu kuyamikila kaamba kolimbikitsidwa kucita ulaliki wa pafoni . Koma anapitiliza kuonetsa kuti anali na “ mtendele wa Mulungu . ” — Afil . ( Chivumbulutso 12 : 7 - 9 , 12 ) Panthawi ino , Satana ni wokalipa kwambili cifukwa adziŵa kuti ali na kanthawi kocepa . Ganizilani munthu amene zokhumba zake zim’pangitsa kucita cinthu coipa cimene anali kuona kuti sangacite . Yehova wa makamu wanena kuti , ‘ Taonani ! Koma kucita zimenezo kukanakhala kunyalanyaza lamulo lake lakuti malipilo a ucimo ndi imfa . Ngati inu nthawi zina mumadzimva conco , mudzalimbikitsidwa kudziŵa kuti mtumwi Paulo anakumana ndi mavuto ofanana ndi anu . Mwina mungadzifunse kuti : N’cifukwa ciani ndifunika kumvetsetsa Baibulo ? Ngati ena mumpingo akonda zosangulutsa zosagwilizana ndi miyezo ya makhalidwe a Yehova , akulu sayenela kulekelela makhalidwe amenewo pofuna kupewa mikangano . ( Sal . 11 : 5 ; Aef . 3 : 21 ) Motelo , pangano la Ufumu linacitidwa ndi Akristu odzozedwa okwanila 144,000 . Mpainiya akuŵelengela Baibulo munthu amene akuyendetsa ngolo mumsewu wa pakati pa mitengo ya Baobab ku Morondava , m’dziko la Madagascar Mofanana ndi munthu amene anapatsa akapolo ake ndalama , Yesu anapatsa otsatila ake odzozedwa nchito yopanga ophunzila . ( Mat . Demetrius ndi anzake ku Karítsa N’ciani cinacitika Aisiraeli atangotuluka kumene mu Iguputo ? Nanga Mose anacita ciani pa cocitikaco ? 33 : 11 . Pamene ndinadziŵa kuti ndili ndi Atate wakumwamba , ndinakhala wofunitsitsa kumudziŵa bwino . Kodi ni banja lanu , nchito yanu , kapena cipembedzo canu ? Kucita zimenezi kudzakuthandizani kudziŵa bwino ‘ malemba oyela amene angathe kukupatsani nzelu zokuthandizani kuti mudzapulumuke . ’ — 2 Timoteyo 3 : 15 . ( a ) Kodi cinali copepuka kwa Hana kukwanilitsa lonjezo lake ? Kodi munthu amene ali ndi nkhawa sangacite ciani ? Baibulo limati maso a Yehova “ ali paliponse . ” ( Miy . Cikondi cake pa Yehova ndi Ufumu wake cinali camphamvu kwambili kuposa zilakolako zathupi . — Maliko 12 : 29 , 30 . Baibo imakamba kuti : “ [ Mulungu ] adzapukuta misozi yonse m’maso mwawo , ndipo imfa sidzakhalaponso . ” — Chivumbulutso 21 : 4 . Kodi akumvetsetsa kuti zimene afuna kucita ni nkhani yaikulu ? Mulungu Wamphamvuyonse , amene analenga cilengedwe conse angakumbukile zonse zokhudza okondedwa athu amene anamwalila kuphatikizapo makhalidwe ao . ( Yes . Ganizilani mmene Yehova anaonetsela kudziletsa pamene Satana anam’pandukila mwamwano . Mtumiki wa Mulungu wokhulupilika anapemphela kuti : “ Tisonyezeni mmene tingaŵelengele masiku athu kuti tikhale ndi mtima wanzelu . ” Mavuto azacuma ndiponso ngongole “ ANA ANU ADZATENGA MALO A MAKOLO ANU ” Kodi cangu ca ophunzila a Yesu cinaonetsa bwanji kuti anali otsimikiza kuti Yesu anaukitsidwa ? Kenako , anati : “ Tabita , dzuka ! ” NYIMBO 11 , 61 Timayesetsa kulimbana nayo ndi mphamvu zathu zonse . Mosayembekezela , banja lathu linasamuka m’dziko la Côte d’Ivoire kupita ku Burkina Faso , ndipo umoyo wanga unasintha kwambili . Mwacitsanzo , ena amatenga loni ya ndalama zambili kuti agulile nyumba , kulipilila ana a sukulu , kugulila galimoto yodula , kapena kuti acitile cikwati capamwamba . Sikuti iye anali kucita zimenezi kuti aoneke kuti ndi wamphamvu . Tinali kucita misonkhano yonse , koma kwa kanthawi tinali kupezekapo anthu aŵili cabe . Yobu akakhala na nkhawa cifukwa coganizila mavuto ake akale , mwacionekele anali kukumbukila uphungu umene Mulungu anam’patsa . Mmene mumalangizila ana anu masiku ano , zidzakhudza mmene adzayamba kucitila akadzakula Musamangoganizila zinthu zimene simungakwanitse kucita koma muzisangalala ndi zimene mumakwanitsa . ” Mabomba anali kumveka akuphulitsidwa m’mwamba zimene zinali kuticititsa mantha kwambili . Mtumwi Paulo anatsiliza mau ake ouzilidwa mwa kunena kuti : “ Zinthu zonse zikadzakhala pansi pake , Mwanayonso adzadziika pansi pa amene anaika zinthu zonse pansi pake , kuti Mulungu akhale zinthu zonse kwa aliyense . ” ( 1 Akor . Miyezi ingapo izi zisanacitike , a Mboni za Yehova anapempha amai kuti aziphunzila nao Baibulo . Kaya tili na ciyembekezo canji , n’cifukwa ciani kuganizila lemba la Aroma caputa 8 n’kopindulitsa ? Timayamikila kwambili thandizo limene Yehova amatipatsa panthawi zovutazo ndi cakudya ca kuuzimu cimene amatipatsa nthawi zonse . Timafuna kuti aliyense azipindula powaseŵenzetsa . Yosimbidwa ndi Adrián de la Fuente Ngakhale zinali conco , Corinna ndi mlongo wina anacita zonse zotheka kuti acoke ku famu ndi kupita kumisonkhano ya mpingo . Kodi wokwela pa hosi yoyela n’ndani ? 5 : 20 - 27 . Kodi tikaŵelenga Baibo , timayesetsa tsiku lonse kusinkhasinkha kapena kuti kuganizila pa zimene taŵelengazo ? Pali mitengo ina ya maolivi imene anthu amanena kuti yakwanitsa zaka pafupifupi 1,000 . Mosiyana na Aisiraeli , ise tili na cifukwa cacikulu cokhulupilila kuti Yehova angaticitile cifundo . Ndipo mogwilizana ndi mau a Yesu , posapita nthawi , iwo anadzionela okha mmene Yehova anayankhila mapemphelo awo . — Mac . Ambili anali kukwatila ndi kusangalala na umoyo wa banja . Analinso kuseŵenza kuti azipeza zofunikila . — Maliko 6 : 3 ; 1 Ates . Cifukwa cacikulu kwambili cimene timalalikilila n’cakuti , timafuna kulemekeza na kuyeletsa dzina la Yehova pakati pa anthu . M’madela ambili anthu amaikila kumbuyo ana acimuna . Iwo amacita zimenezi cifukwa coganiza kuti anawo akadzakula adzapitiliza ndi dzina la banja , ndi kusamalila makolo okalamba ndi ambuye ao . ( Chiv . 20 : 2 , 3 ) Cifukwa cakuti Mdyelekezi ndi ziŵanda zake sadzakhala ndi mphamvu , anthu a padziko lapansi adzakhala ndi moyo popanda cisonkhezelo ca Satana ndipo adzakhala ndi mwai wogonjela kothelatu Mfumu yao yaulemelelo ndi yopambana . Umaposa Kuganiza Mozama Kulikonse , ” Aug . Mofanana ndi Atate wake , Yesu nayenso anali kumvela cifundo anthu amene anali na njala yauzimu . Chivumbulutso 6 : 3 , 4 Timayamikila Yehova cifukwa cotipatsa ciyembekezo cakuti tidzauka . Pa cocitika cina , Yosefe anapelekanso citsanzo cabwino ca kudziletsa . Izi zimatitsimikizila kuti iye ni wofunitsitsa kukwanilitsa malonjezo ake onse . Akulu amenewa ndi abusa auzimu odzicepetsa . ( a ) Kodi Yesu anali wokongola pa zifukwa ziti ? Mboni zimacita zimene zingathe kuti zilalikile uthenga wabwino kwa anthu amene amakamba Ciwayu . 8 : 9 , 13 ; 10 : 32 ) Kumaiko ena , kusunga ndevu si kofala ndipo si kololeka kwa Mkhiristu . Ndiponso kungakhale cifukwa comunenezela . Kodi n’ciani cimene anaona m’masomphenya ake a namba 7 ? Ndinali kusangalala kwambili ndi kuphunzila kumeneko . Ife anthu mwacibadwa timafunitsitsa kupitiliza kukhala na moyo . Monga mmene munthu wakhungu sangaonele mthunzi kapena dzuŵa , ndi cimodzimodzinso ndi ife , Yehova sitingamumvetse patokha . 12 : 12 ; 1 Akor . 16 : 19 ) Masiku ano , anthu a Mulungu padziko lonse lapansi amasonkhana m’Nyumba za Ufumu masauzande ambilimbili kuti aphunzile Baibulo ndi kulambila Yehova . Makolo ena ku United States anathandiza ana awo kukhala na zolinga zauzimu . Ine ndi Jenny ku Tuvalu Zitsanzo zimenezi “ zinalembedwa kuti zitilangize . ” “ Peleka nchito zako kwa Yehova , ndipo zolinga zako ndithu zidzakhazikika . ” — MIY . Yehova akuti : “ Ine ndimakhala kumwamba pamalo oyela . Ndimakhalanso ndi munthu wopsinjika ndi wa mtima wodzicepetsa , kuti nditsitsimutse mtima wa anthu onyozeka ndiponso kuti nditsitsimutse mtima wa anthu opsinjika . ” — Yesaya 57 : 15 . Mosiyana ndi mapangano ena , Yehova alibe mbali m’pangano limeneli . M’malo mwake , pangano limeneli lili pakati pa Yesu ndi odzozedwa . Iye anati : “ Panthawiyo tinakondwela kwambili . Mlongo wina dzina lake Annette anati : “ Ngati okwatilana sakhululukilana , mkwiyo ndi kusadalilana zimakula . Nthawi zambili tinali kugula zinthu zimene sitinafune kugula . Warren , amene wathandiza abale ambili kupita patsogolo kuuzimu anafotokoza cifukwa cake . Iye anati : “ Kuti wina ayenelele kukhala mkulu payenela kupita nthawi . N’nali kuphunzila zoimba - imba pa sukulu inayake , kuti mwina nikapite ku yunivesite , cifukwa n’nali kufunitsitsa kudzakhala katswili woimba . Nimurodi anali “ mlenje wamphamvu wotsutsana ndi Yehova . ” Mulungu amaona ciliconse , ndipo palibe cimene cingamulepheletse kuona zoipa zimene munthu amacita ngakhale atabisa bwanji . M’zaka za m’ma 1700 , akapolo a m’dziko la Hispaniola , limene ndi cisumbu panyanja ya Caribbean , anaukila mabwana awo . Wodala ndi iye wobwela m’dzina la Yehova . ” Kodi n’kutheka kuti pamene Mose anamenya thanthwe m’malo mongokamba nalo , anapangitsa anthu kukayikila kuti Yehova wacita cozizwitsa ? Ena amacita nayo cidwi . Ndinatengela kapesedwe kake ka tsitsi , kayendedwe kake ndi mmene anali kukuwila akamacita masewela oponya zibakela . Mosakayikila , mungatelo . Nanga kodi paradaiso ingakhaledi yeni - yeni ? ’ Ziwiya zoonetsela mafilimu zochipa zinali kupezeka ndi Ophunzila Baibulo . Iye anati : “ Mu 2014 , n’napezeka pa msonkhano wacigawo wapadela mu mzinda wa Yangon . Kumeneko n’nakumana na banja linalake limene linali kutumikila m’gawo losoŵa la Cichainizi mu Myanmar . Kodi Mkristu wofikapo amawaona bwanji malangizo ndi mfundo za Mulungu ? 13 : 5 , 6 . 20 , 21 . ( a ) Kuganizila mozama za dipo kudzatithandiza motani kugonjetsa maganizo olefula ? “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , . . . amatitonthoza m’masautso athu onse . ” — 2 AKOR . Kodi iye amakhulupililadi kuti Yehova adzaukitsa mwana wake ? Kaamba ka ici , iwo amafunika kulimbikitsiwa . Kudalila Mulungu kumatithandiza kukhala ndi cikhulupililo ndiponso wolimba mtima tikakumana ndi mavuto . Cifukwa ca makonzedwe amenewa , abale na alongo ambili apeza mabwenzi atsopano ndipo ni ofunitsitsa kudziŵana ndi Akhristu a zikhalidwe zosiyana - siyana . ( a ) Kodi mtumwi Paulo anaonetsa bwanji kuti anali kuona moyo mmene Mulungu amauonela ? Pa cifukwa cimeneci , tili ndi udindo wophunzitsa ena mmene Yehova akuonetsela cikondi cake ndi mmene iwo angapindulile . 4 : 23 . Tsiku lina , Yehova anakamba ndi mtumiki wake wokhulupilika ameneyo . Tiyenela kuliona bwanji lamulo la Yehova lonena za magazi ? Mlongo Ishii ndi mlongo wina wacikulile dzina lake Sakiko Tanaka , anali kuvala zovala zaulemu zooneka ngati khoti kuti akalalikile kwa akuluakulu a boma . Mafunso amenewa angakuthandizeni kutsatila malangizo a Paulo akuti : “ Muzindikile cimene cili cifunilo ca Mulungu , cabwino , covomelezeka ndi cangwilo . ” Iye anakhala ndi moyo mogwilizana ndi dzina limene Mulungu anam’patsa , lakuti Yesu . ( 1 Akor . 7 : 27 ) Paulo anakamba izi cifukwa anali kudziŵa kuti Yehova amadana ndi anthu amene amathetsa cikwati mwacinyengo . — Mal . Mufunika kukhala wolimba mtima kuti mukwanitse kukana mapempho obweleza - bweleza amenewo , ndi kupeleka citsanzo cabwino kwa ana anu . Masiku ano , kodi abale a m’Makomiti ya Nthambi , amadela , ndi akulu mumpingo , ayenela kucitanji akalandila malangizo a gulu la Mulungu ? Timakhala ndi mtendele wamaganizo ngati makolo athu asamalilidwa bwino . Baibulo limatiuza kuti anthu okhwima kuuzimu anaphunzitsa “ mphamvu zao za kuzindikila ” kuti azisiyanitsa cabwino ndi coipa . Funso lacitatu n’lakuti , ngati mau a Yesu onena za cikwati pambuyo pa ciukililo akamba za ciukililo ca kumwamba , kodi zimenezi zitanthauza kuti aja amene adzaukitsidwa padziko lapansi adzayamba kukwatila ? Kuti munthu alemekeze wina , afunika kudziŵa mmene munthuyo amaonela zinthu . Anthu ambili amene amaphunzila Baibulo afika pokamba mau amene mtumwi Paulo analemba akuti : “ Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu . ” Kupanduka kwa Satana sikunaletse Yehova kuonetsa cikondi ku mtundu wa anthu , kapena kulepheletsa anthu opanda ungwilo kukhala okhulupilika kwa Yehova . Petulo ayenela kuti anali ndi maganizo abwino ndithu ponena zimenezi . Nthawi yabwino yocita mdulidwe . 7 : 45 - 49 ; 9 : 22 ) Munthu akacotsedwa m’sunagoge anali kunyozewa , kusankhiwa , ndi kukaniwa na Ayuda anzake . Ni vuto lanji limene mbale Robert anali nalo mu umoyo wake wauzimu ? Nanga anacitapo ciani ? Ngati ndinu m’bale wobatizidwa , kodi ‘ mukuyesetsa ’ kuti muyenelele kukhala mtumiki wothandiza kapena mkulu kuti muzitumikila abale ndi alongo mumpingo wanu ? — 1 Timoteyo 3 : 1 . Mau amenewo anali akuti : “ Tsiku lina dziko lidzatha . ” Kuopa Mulungu kumaticititsa kuti tisamaope anthu . ( 1 Sam . 23 : 15 . Kutumikila Yehova si kolemetsa kwa anthu amene amamukonda . M’bale Donald , amene watumikila monga mkulu kwa zaka zambili , anati : “ Amuna a paudindo afunika kumalimbitsa ubwenzi wawo na Mulungu . Ngakhale kuti Adamu ndi Hava analephela kugwila nchito imene anapatsidwa , anthu ambili anagwila nchito imene Mulungu anawapatsa . ( Gen . Wamasalimo anaimba kuti : “ Taonani ! N’zoona kuti sitingathetse cisoni conse cimene munthu amakhala naco ngati wokondedwa wake wamwalila . Koma tingathe kum’tonthoza mwa kuyesetsa kumuthandiza m’njila zosiyana - siyana . ( 1 Yoh . ( 1 Mbiri 17 : 16 ; 2 Mbiri 30 : 27 ; Ezara 10 : 1 ; Machitidwe 9 : 40 ) Iye safuna kuti tikhale mwanjila inayake yapadela popemphela . Conco , Yehova anamukhululukila ndipo anapitiliza kumuseŵenzetsa . Ngati tipilila tidzalandila mphoto . ( Aheb . 13 : 5 , 6 ) Kodi tingatsatile bwanji malangizo amenewa ? Nili m’timu imeneyi , munthu wina ananipempha kuyenda ku Nicaragua kukagwilizana ndi timu ya akatswili pa maseŵela amenewa . Apo n’kuti nili na zaka za m’ma 20 . Yesani kudziŵa mmene akumvelela . “ Kulambila kwa Pabanja kumathandiza munthu kuyandikilana ndi banja lake ndi Yehova . Palibe vuto limene Yehova angalephele kuthetsa . N’nafika ku Beteli pa June 19 , 1950 , ndipo n’nayamba kugwila nchito imene n’napatsidwa . Akristu acikulile ali ndi luso lofunika pothandiza anthu a Yehova mwa kuphunzitsa , kutsogolela , ndi kulimbikitsa abale ndi alongo . — Ŵelengani Yobu 12 : 12 . Malangizo a Mulungu ndi ozikidwa pa cikondi , ndipo iye amatilanga cifukwa ca cikondi cimeneci . Conco , ngati titenga cakudya cathu cauzimu , koma kucokela ku magwelo ena , tingadye cakudya coipitsidwa . — Sal . Pakuti ayenela kulamulila monga mfumu kufikila Mulungu ataika adani onse pansi pa mapazi ake . Ngati tifuna kuti tikapindule ndi madalitso amenewa , tiyenela kupitiliza kukula kuuzimu ndi kuyendela limodzi ndi gulu la Mulungu nthawi zonse . Nkhani ziŵilizi zifotokoza mmene kukambilana ndi Yehova ndiponso kumudalila nthawi zonse kumalimbitsila ubwenzi wathu ndi iye . Munthu wokhulupilika , Yobu . Paulo anagwila mau a Yesu akuti : “ Taonani ! Tikatelo ndiye kuti tikukonzekela kudzakhala m’dziko latsopano . Cimodzi mwa zinthu zoyambilila zimene tinaphunzila , ni ulosi wa pa Genesis 3 : 15 . Kodi anthu odzikonda amacita zinthu motani ? Tiyenela kupemphelela abale , alongo , ndiponso ana amene ali m’ndende m’dziko la Eritrea MFUNDO YA M’BAIBO : “ Phunzitsa mwana m’njila yomuyenelela . Chulani njila imodzi imene tingaonetsele kuti timamuyamikila Yehova potilola kukhala naye pa ubwenzi . Nanga Yesu anacita bwanji zofanana ndi zimenezi ? ( Aheb . 13 : 18 ) Popeza kuti timafunitsitsa “ kucita zinthu zonse moona mtima , ” timapewa kudyela masuku pamutu abale athu . Pamene alengezi a Ufumu akuonjezeleka , ndiponso pamene tikuyandikila mapeto a dongosolo lino , nchito yomanga idzapitilizabe . ( Yes . Iye sanali kufuna kuti anthu azimutama . Ife anthu tinalengedwa m’cifanizilo ca Mulungu . Tiyeni tonse tipitilize kufunafuna cidziŵitso , kumvetsa zinthu , ndi nzelu . 116 : 12 , 14 . ( Ŵelengani Yuda 20 , 21 . ) ( Deuteronomo 24 : 6 ) Mulungu anaona kuti mphelo inali yofunika kwambili cifukwa popanda iyo , banja silikanapanga mkate wao wa tsiku ndi tsiku . — Onani kabokosi kakuti “ Kupela ufa ndi Kuphika Mkate wa Tsiku ndi Tsiku m’Nthawi za m’Baibulo . ” MKATE WOKHUTILITSA MTIMA WA MUNTHU Ngati timakhululukila ena , timaonetsa kuti ndise anthu okhazikitsa mtendele . Nanga n’cifukwa ciani anasintha ? Zaka zapitazo , mzimayi wina amene tam’patsa dzina lakuti Rose anamvela uthenga wa Ufumu . Ndipo popemphela kwa Yehova , n’nali kuyamba mwa kupepesa pa zimene n’nacita . ” ( Ŵelengani Aheberi 6 : 1 . ) Ndipo mu 2015 cabe , anthu amene anathaŵa kwawo anali pafupi - fupi 12.4 miliyoni . ( 2 Akor . 6 : 3 ) Ngati timalemekeza nyumba ndi katundu wa anthu a m’gawo lathu , io angalandile coonadi . — Ŵelengani 1 Petulo 2 : 12 . ANTHU ambili ogwila nchito zacipatala amaseŵenza pakati pa anthu odwala matenda oyambukila . N’ciani cingakulimbikitseni kuphunzila cinenelo cina ? Pa nthawi ina , anaphunzitsa khamu la anthu pa Ulaliki wake wochuka wa pa Phili , ndipo “ khamu la anthulo linakhudzidwa moti linadabwa ndi kaphunzitsidwe kake . ” Mafumu acikanani anagwilizana ndi Mfumu Yabini amene anali wamphamvu kwambili kuposa mafumu onse . 22 M’dziŵeni Mdani Wanu A Mboni za Yehova angakuthandizeni kudziŵa bwino coonadi ca m’Baibulo . Mtumwi Paulo anali mmodzi wa anthu olimba mtima ndiponso ‘ odziŵika ndi dzina [ la Yehova ] ’ m’nthawi ya atumwi . Amaganiza kuti Mulungu sakhudzidwa ndi zimene zimawacitikila pa umoyo wao . Koma Asamariya sanawalandile . Conco , Yakobo na Yohane mwaukali anapempha Yesu kuti awalole kuitana moto kucokela kumwamba kuti unyeketse mudzi wonse . 4 : 13 ) Khalidwe la tsankho limene anthu anaonetsa kwa Yesu na ophunzila ake , linayamba cifukwa ca kusiyana kwa zipembedzo , cikhalidwe , na mitundu . ( Chiv . 20 : 7 - 10 ) Satana alibe ciyembekezo ciliconse , koma ife tili ndi ciyembekezo ca tsogolo labwino . Ezekieli anaona masomphenya amenewa mu 612 B.C.E . Atatsiliza kukambilana , sipanapite nthawi yaitali kuti Nikolai aitanidwe ku likulu la apolisi , ku tauni ya Kant . ( Luka 14 : 33 ) Pemphani akulu kuti akuthandizeni , ndipo tsatilani malangizo a m’Baibulo amene io angakupatseni . Kugwila nsomba ndi neti kumafuna mphamvu , mgwilizano ndiponso anthu ambili . — Luka 5 : 1 - 11 . 7 : 1 - 4 ) Nanga Yesu anali kukamba za kusonkhanitsa kuti ? Pokumbukila zimene zinacitika , Mlongo wina amene anapulumutsidwa pamodzi ndi mwamuna wake ananena kuti pamene ngalawayo inali kumila mayi wina anali kulila uku akukuwa kuti : “ Masutikesi anga ! Conco , iye anasankha kumvela mau a mkazi wake kuposa mau a Yehova , Mulungu wake . — Gen . ( b ) Kodi pakubuka mafunso ati ? Pamene anali kuvutika , sanaopseze . ” “ Ine na amuna anga sitimakakamiza ana athu kucita zinthu zimene ise sitimacita . ” — Christine . Cimakwilila zinthu zonse , cimakhulupilila zinthu zonse , cimayembekezela zinthu zonse , cimapilila zinthu zonse . Kodi ndinu mkulu mumpingo kapena woyang’anila dela ndipo mumapanikizika cifukwa ca kuculuka kwa maudindo ? Cigumula citatha , Yehova analamula anthu kuti asamadye kapena kumwa magazi . Ndiyeno tingafunse kuti : “ Bwanji ngati mwadziŵa kuti mwana wanu amasonkhezeledwa ndi munthu wina woipa kwambili ? ” Ndinakumbukila kuti pamene ndinali mwana atate anandiuza kuti ndiyenela kuŵelenga Baibulo . Yoyamba , mayeselo amene timakumana nawo ‘ amagwelanso anthu ena . ’ Kodi amayi ake angam’lange bwanji ? Ni vuto lalikulu liti limene Yosefe anakumana nalo ? Nanga citsanzo cake n’colimbikitsa bwanji kwa ife ? Yehova watilonjeza kutipatsa zinthu zofunikila ngati timamukhulupilila ndi kuika Ufumu wake pamalo oyamba . Cikondi cimene Yehova amationetsa ndiponso cikondi cathu pa iye zimatipatsa cimwemwe ceniceni . 43 : 30 , 31 ; 45 : 1 ) Ngati Mkhristu mnzanu kapena munthu wina amene mumakonda wakulakwilani , mungacite bwino kutengela citsanzo ca Yosefe . Lothela , ngati Akhiristu analoŵa mu ukapolo ku cipembedzo conama m’zaka za m’ma 100 C.E . kupita m’tsogolo , kodi anamasukamo liti ? Kodi misonkhano yathu imathandiza bwanji kuti tizilimbikitsana wina na mnzake ? 32 : 7 - 14 . Ofalitsa ena amakhala ndi magawo aakulu osavuta kulalikilamo . Pa cifukwa cimeneci , io amacita mantha kuti mwina angalephele kumaliza kulalikila gawo lonse . Muuzeni kuti ndinu ndani , ndipo mvetselani mwaulemu olo kuti wodwalayo akuoneka kuti wasokonezeka . Iye akhoza kuona kuti mwamuna wakeyo samukonda ndipo salemekeza makonzedwe a ukwati . — Mateyu 5 : 28 . EUROPE : Mmodzi wa akuluakulu a bungwe la European Commission , amai Cecilia Malmström , anakamba kuti : “ Vuto limeneli [ la ziphuphu ] ku Europe lafika poipa kwambili . ” Kodi wacicepele ayenela kukumbukila ciani pokambilana na ŵena za Mulungu na cilengedwe ? ( 1 Akor . 5 : 11 ; 2 Yoh . Mu 1949 , ku Hemsworth , titangokwatilana kumene Mwacitsanzo , ambili alibe mavidiyo ndi nkhani zina zimene zimapezeka cabe pa jw.org . POPEZA tikhala m’dziko la mavuto , pamafunika khama kuti tipeze mtendele . Posafuna “ kudzionetsela , ” ndinali kuyenda pansi kupita ku nyumba imene andikonzela , m’malo mokwela takisi . Pamene Marita anatangwanika na kukonza cakudya , Mariya anakhala pafupi na Yesu n’kumamvetsela zokamba zake . ( Ŵelengani 1 Yohane 5 : 19 . ) Koma amene atumikila ku gawo la cinenelo cina amakumana na mavuto ena . Pogwilitsila nchito mkate wopanda cotupitsa ndi vinyo wofiila , iye anayambitsa cimene cimachedwa kuti Cakudya ca Madzulo kapena kuti Mgonelo wa Ambuye ndipo anawauza kuti : “ Muzicita zimenezi pondikumbukila . ” — Luka 22 : 19 . 17 : 5 - 8 . ( Mateyu 24 : 14 ) Kodi mudziŵa kuti ophunzila a Khristu akugwila nchitoyi motsogoleledwa na angelo ? Komabe , tingafunse kuti : Kodi lonjezo n’ciani ? 3 : 7 - 10 ) Komabe , tifunika kuwathandiza ndithu . Izi zingakhale zokhumudwitsa . Nanga n’zitsanzo ziti zakale na zamakono zimene zingatilimbikitse ? N’cifukwa ciani Akristu ambili anali kukamba Cigiriki ? Kodi mfundo imeneyi itiphunzitsa ciani za Yehova ? Ni makhalidwe ena ati amene tifunika kuleka ndi kupitiliza kuwapewa ? Don anafotokoza zokhudza mmodzi wa anthu amenewa . Iye anati : “ Peter anali mmodzi wa anthu adothi kwambili okhala m’miseu . Tili ndi udindo wolalikila uthenga wabwino kwa anthu padziko lonse lapansi . Pa cifukwa cimeneci , timamasulila zofalitsa zathu m’zinenelo zoposa 700 . ( Genesis 12 : 5 ) Mosakaikila , Abulahamu na Sara anali kuuzako anthu ofuna kumvetsela za cikhulupililo cawo . Kodi mwatsimikiza mtima kucita ciani pofuna kuonetsa kuti mumakonda utumiki wopulumutsa moyo ? Kukwanilitsa zolinga kungakuthandizeni kuti musamadzikayikile , mulimbitse maubwenzi anu , ndiponso muwonjezele cimwemwe canu . Mwacitsanzo , kodi mumamva bwanji mukaganizila mmene Yehova anacitila zinthu ndi Mfumu Azariya ya Yuda ? Malo olambilila : Zaka zapakati pa 100 B.C.E . ndi 300 B.C.E . , olemba Pentatuke ya Asamariya anawonjezelapo mawu ena pa Ekisodo 20 : 17 akuti “ ku Gerizimu . APAINIYA Kodi anthu okhulupilika amene anali na moyo m’nthawi imene Mulungu sanali kuukitsa akufa , anali naco cikhulupililo cakuti Mulungu adzaukitsa akufa m’tsogolo ? 1 : 8 ) Cifukwa cakuti anali ‘ kuŵelenga mau a Yehova ’ m’cinenelo cakwawo , Danieli anakhalabe wolimba mwauzimu pamene anali ku dziko lacilendo . ( Dan . Anataya ciyembekezo cokhala na moyo wosatha m’Paradaiso padziko lapansi . — Genesis 2 : 17 ; 3 : 1 - 6 ; 5 : 5 . 6 : 13 ) Kukamba zoona , nthawi zina pamafunika kulimba mtima kuti tikhale “ mboni yokhulupilika ndi yoona ” m’dziko lodzala cidani la Satana . — Chiv . Popeza ciletso cinali cikali mkati ku Romania , tinali kukumana mwakabisila m’nyumba ya M’bale Pamfil Albu , pamodzi ndi abale anai audindo ndi oimila Komiti ya Dziko . Iye anati : “ Mu 2004 banja lina limene linali kutumikila ku Belize linanipempha kuti nikawacezele ndi kucita nawo upainiya kwa mwezi umodzi . Mwacionekele , mumamuyewa wokondedwa wanuyo . Ndiyeno , a tica anauza anawo kuti akapita ku nyumba , aliyense wa iwo akatambe vidiyo ya zithunzi zodrowing’a yakuti , Kugonjetsa Munthu Amene Akukuvutitsani Popanda Kumenyana Naye . Pamene maso ake “ akuyendayenda padziko lonse lapansi , ” iye amadziŵanso anthu amene mitima yao si ‘ yanthunthu kwa iye . ’ Mmene Mulungu amacitila zinthu zimasiyana kwambili ndi anthu . Pamene anali kukamba za tsiku la Nisani 14 , caka ca 1513 B.C.E . , Mose anati : “ Zaka 430 zimenezi zitatha , pa tsiku lomwe zinatha , makamu onse a Yehova anatuluka m’dziko la Iguputo . ” ( Eks . M’malomwake , ndidzalibweletsa panyumba yake m’masiku a mwana wake . ” Delphine anati : “ M’maganizo mwanga , nimayelekezela kuti nikumuona mwana wanga ataukitsidwa . 72 : 7 ) Ndithudi , cilango ca Yehova cimatikonzekeletsa kudzakhala na moyo wosatha mwamtendele ndi mogwilizana , monga banja lake losamalidwa mwacikondi . Tiyeni tikambilane zitsanzo zina za m’Baibulo zimene zidzatithandiza kuona ubwino woyamikila colowa cathu cakuuzimu . ( a ) Kodi Yesu wakhala akukonzekeletsa bwanji mkwatibwi wake wamtsogolo ? Zimenezi zinandikondweletsa kwambili ! ” 21 : 10 - 14 . Kodi zimenezi zitanthauza ciani ? * Cikumba naconso cimadyewa na tuzilombo . ( Yohane 17 : 17 ) Kuti titengele Yesu , tifunika kuŵelenga Baibulo tsiku ndi tsiku , kuliphunzila , ndi kusinkhasinkha zimene taphunzila . Motelo , n’ciani cidzacitikila osakhulupilika amenewo ? M’nkhani ino ndi yotsatila , tidzaphunzila mmene Yehova kwa zaka zambili wagwilitsila nchito amuna ena kuti atsogolele . Komabe , ngati ndinu a “ khamu lalikulu ” la “ nkhosa zina , ” Mulungu wakupatsani ciyembekezo ca padziko lapansi . ( Chiv . ( Chivumbulutso 6 : 2 ) Kodi Yesu anaikidwa liti kukhala Mfumu kumwamba ? Tsiku lililonse abale amatisamalila mwacikondi . Kenako anali kupitila limodzi ndipo m’njila anali kuthandizana . M’masiku otsiliza ano , odzozedwa apitilizabe kukhala maso . Ena amacotsedwa nchito ndipo amasoŵa njila ina yopezela ndalama . Ambili mwa acicepelewo amasonkhana ndi kulalikila . Khalidwe lake . Woyang’anila nchito wina wa ku Hawaii , U.S.A . , analemba kuti : “ Sitinadziŵe kuti tumapepala tumenetu tudzakhala tothandiza mu ulaliki wa kunyumba ndi nyumba , ndi wa mu mseu . ” Komabe , mayeselo a Rudolf anali asanathe . Iye anati “ Kunena zoona kuika maganizo pa utumiki kwandithandiza kwambili kuthetsa vuto limenelo . N’ciani cingatithandize kupanga zosankha zabwino ? Kuti muyambe kuona nchito moyenela , mungacite zotsatilazi : ku sukulu ? Conco , anapeleka ang’ono anga , Araceli , Lauri , ndi Ramoni kunyumba ya masisitele mumzinda wa Bilbao kuti azikakhala ndi masisitele . Tingaonetse bwanji kuti tikukonzekela kudzakhala ndi moyo wosatha m’Paladaiso ? Mwacitsanzo , uthenga wa Ufumu unafika m’dziko ka Cuba mu 1910 , ndipo M’bale Russell anapita kukaceza m’dzikolo mu 1913 . Kagulu ka Ayuda omenyela ufulu wa dziko lawo , kochedwa Azeloti , kanali kulimbikitsa anthu kukhala na maganizo amenewa . N’cifukwa cake Paulo analembela Timoteyo kuti : ‘ Ndimakumbukila misozi yako . ’ Timayamikila kwambili kuti Yehova wakhazikitsa atumiki ake masiku ano monga mmene anacitila m’nthawi zakale . ( Yesaya 9 : 6 ; Salimo 46 : 9 ) Baibulo limati : “ Mulungu adzakhala woweluza pakati pa mitundu yambili ya anthu . . . Ndinalimbikitsidwa kwambili kutumikila pamodzi ndi Anthony Conte . Iye anali m’bale wokoma mtima , waluso ndi wokonda utumiki . Nanga bwanji ngati mufuna thandizo kuti mumvetse na kuseŵenzetsa malangizo a m’Baibo ? ( Zek . 5 : 4 ) Lumbilo ni mau amene munthu amakamba pofuna kutsimikizila kuti zina zake n’zoona , kapena ni lonjezo lakuti munthu adzacita kapena sadzacita zinazake . Pokamba za kubwezeletsa Yerusalemu , wamasalimo anaimba nyimbo yotamanda Yehova . Iye anati : “ Walimbitsa mipilingidzo ya zipata zako . Wadalitsa ana ako amene ali mwa iwe . Tidzasangalala kwambili ndi zinthu zabwino zimene tinalonjezedwa , koma madalitso aakulu amene tidzalandila ndi akuuzimu . Mkaziyo anali Abigayeli . Mlongo wina anaseŵenzetsa tumabuku tuŵili tumene tatomola m’ndime 5 pokambilana na mnyamata wina amene anayamba kukhulupilila za cisanduliko cifukwa coganiza kuti Mulungu kulibe . Mwacitsanzo , zimene wina angakambe zingatikhumudwitse kwambili . Kodi muganiza kuti ngati mwamuna ndi mkazi agwilitsila nchito malangizo amenewa angakhale ndi banja lacimwemwe ? ( Mateyu 10 : 8 ) Conco , nchito yolalikila siyenela kukhala bizinesi . Kuonjezela apo , mzimu woyela ungatipatse mphamvu kuti tipewe kuumbidwa ndi dziko loipali . A Inoki : Cabwino , kodi simukuvomeleza kuti mwamuna amafuna kulemekezedwa ndi mkazi wake ndiponso mkazi amafuna kuti mwamuna wake azionetsa kuti amamukonda kwambili ? 1 , 2 . ( a ) Kodi atsogoleli acipembedzo anali kufuna kudziŵa ciani ? Nanga Petulo anayankha motani ? Cocitika cimeneci cinali colimbitsa cikhulupililo ngako ! — 2 Mbiri 5 : 13 , 14 ; 7 : 6 . Paulo anakamba kuti mzimu umenewu , kapena kuti ‘ kaganizidwe kameneka tsopano kakugwila nchito mwa ana a kusamvela . ’ ( Aef . Koma io akudziŵa kuti adzakhala olamulila anzake a Yesu mu Ufumu wakumwamba ngati akhalabe okhulupilika mpaka imfa . Cimwemwe cotelo siticita kubadwa naco ndiponso sicibwela cokha . David : Kutumikila Yehova kwasintha kwambili umoyo wathu . Abale amenewo anatengela citsanzo ca Yesu . Cotelo , ndinaleka kupita ku chechi . Ufumu wa Mulungu ukadzabwela , sikudzakhala kulipila malendi kapena kutenga nkhongole . Cakudya cidzakhala camahala ndi ca mwanaalilenji . Nkhanizi zikufotokoza zozizwitsa za Yesu . Zikutiphunzitsa kukhala oolowa manja ndi kukhala ndi mtima wofuna kuthandiza ena , ndiponso zikufotokoza mbali zocititsa cidwi za umunthu wake . Pangano la Abulahamu linayala maziko a zonsezi . 3 : 18 - 21 . M’malo mwake , tiyenela kukulitsa cikondi cathu pa Yehova . Pa zinthu zam’mabwinja zimene zinafukulidwa ku Middle East , panali miyala imene inali kugwilitsidwa nchito pomenya nkhondo ndi gulaye m’nthawi zakale . Tiyenelanso kuzindikila nthawi imene tikhalamo na zimene zicitika , kuti tikonzekele zimene zidzacitika posacedwa . ( Chiv . MATENDA , KUVUTIKA , NA IMFA , ZONSE ZIDZATHA : “ Cihema ca Mulungu cili pakati pa anthu . . . Kodi Yehova anaiŵala zimene analonjeza Abulahamu ? ( b ) Kodi adani athu adzamva bwanji ? Masisitele sanandilimbikitse kukatumikila Mulungu ku dziko lina monga mmene ndinali kufunila . Mwacitsanzo , Malemba amatiuza mmene anali kucitila zinthu ndi Aisiraeli ngakhale kuti nthawi zambili io sanali kumumvela . Yehova anaika Mwana wake monga Mfumu Mesiya kumwamba mu 1914 . Nanga ndalama zocitila zonsezi timazipeza bwanji ? Cifukwa ca cizunzo , Tyndale anacoka ku England ndi kupita ku Ulaya kuti akamasulile ndi kusindikiza Baibulo . Senakeribu , Mfumu ya Asuri , anatonza Yehova ndi kuopseza Hezekiya n’colinga cakuti angodzipeleka m’manja mwawo . Koma inapitiliza kunena kuti , “ Mboni za Yehova sizivala conco . . . . Ngati tifuna kusankha zocita pankhani inayake , pangakhale zosankha zingapo zimene tingapange patokha zovomelezeka kwa Yehova . N’cifukwa cake iye anati : “ Ine ndi amene ndimanena za mapeto kuyambila pa ciyambi . Kuyambila kalekale , ndimanena za zinthu zimene sizinacitike . ” M’dziko lino la ciwelewele , zingakhale bwino ngati onse a m’cikwati akanakhala okhulupilika conco . Koma masiku ano iwo amavomeleza kuti cilengedwe cinali na ciyambi . A Daka : N’cifukwa ciani mumakonda kukamba za Yehova ? Nanga bwanji ngati mukudziimba mlandu ? Mungadziŵitsenso amene anali kusamalila wodwalayo ndi acibale kuti wamwalila , ndi kuti sakuvutikanso . Amayi anayesetsa kuniletsa kuyanjana ndi a Mboni , koma panthawiyi n’nali wotsimikiza mtima kupanga coonadi kukhala canga . Masiku ano , kuwala kwa coonadi kwaonjezeka , ndipo ise tingathe kum’dziŵa bwino kwambili Mulungu kuposa mmene amuna amenewa anam’dziŵila . ( Miy . N’nakhala memba wa gulu landale la acicepele lochedwa Free German Youth limene linali kucilikizidwa na boma . N’zoona kuti kuphunzila Baibulo kungakhale kovuta kwa ambili a ife . Onani zitsanzo ziŵili zotsatila : Nimakhala wacimwemwe ngako pamene niwathandiza kudziŵa Yehova . Pamene tilalikila , timathandiza anthu kupindula na uthenga wathu wa mtendele wokamba za Ufumu wa Mulungu . ( Yes . 9 : 6 , 7 ; Mat . Kodi Mau a Mulungu ali na malangizo otithandiza za conco zikaticitikila ? Koma zoyesa - yesa za Satana sizingaphule kanthu . Komabe , Mulungu “ anatikonda ndi kutumiza Mwana wake [ Yesu Kristu ] monga nsembe yophimba macimo athu . ” Kodi zimene zinalembedwa m’mauthenga amenewo zinacitikadi ? Onani mfundo zisanu zimene zathandiza anthu ambili . 11 : 9 ) Ni vuto lanji limene lingakhalepo ngati timangotsatila mtima wathu pocita zinthu ? Ndipo munapitiliza kufufuza kuti mupeze cuma cina ca kuuzimu . Ndipo apainiya ambili acicepele amayenda kumalo osoŵa kapena kudela kumene akamba cinenelo cina kuti akalalikile uthenga wabwino . Pambuyo popatsidwa cilangizo cofunikila , anthu oyeletsedwa a Yehovawo anakhala okonzeka kulandilanso utumiki wina watsopano . Ndipo sitiyenela kudabwa kuti nthawi zina atumiki ena a Yehova angakhale ndi cakudya ca kuuzimu coculuka kuposa ena . Nthawi zambili n’nali kufunsila malangizo kwa iye na kuwaseŵenzetsa . Apainiya amenewa ni ogalamuka m’njila yakuti amaona utumiki wa nthawi zonse kuti ni nchito yofunika mu umoyo wawo wonse . Mosakaikila cifundo cimene cinam’cititsa kuukitsa mwana wa mkazi wamasiye , ndi cimene cinam’cititsanso kuukitsa Lazaro . Mu 1943 , abale na alongo ku Mexico anavala zikwangwani polengeza za msonkhano wadela wa mutu wakuti “ Mtundu Waufulu , ” umene unacitikila m’mizinda 12 ya m’dzikolo . 2 : 17 ) Kodi tiphunzilapo ciani pa colakwa ca Mose ? ( Miy . 8 : 30 ) Kupyolela mwa iye , Yehova analenga zolengedwa zina zauzimu mamiliyoni ambili kumwamba . Ena amayamba kulambila kwa pabanja mwa kuimba nyimbo zotamanda Yehova . Koma maulendo opita ku madoko ndi ku positi ofesi ananithandiza kukhala wolimba . M’kupita kwa nthawi , banjali linathandiza kuti mpingo wa Cipwitikizi ukhazikitsidwe . Kunena zoona m’baleyo adzalimbikitsidwa kwambili ndi pemphelo lanu locokela pansi pamtima . Zinakonzewa m’njila yakuti zikuthandizeni kuganizila mozama zimene mumakhulupilila , cifukwa cake mumazikhulupilila , na mmene mungafotokozele zikhulupililo zanu kwa ena . 5 : 23 , 24 . Kupanga zida za nkhondo kumalila ndalama zambili komanso luso . Kukanakhala kuti ndalama zonsezi amaziseŵenzetsa pothandiza anthu , kodi zinthu sembe zili bwanji padziko ? Kodi mukumbukilako zida zina zimene zilipo m’citundu canu ? ( Mlaliki 3 : 11 ) Olo kuti patekha sitingakhutilitse colaka - laka cimeneci , dipo imacititsa zimenezi kukhala zotheka . Anafunika kumvela Mulungu . ( 2 Mbiri 32 : 24 - 26 ) Kukamba zoona , Hezekiya ndi citsanzo cabwino cimene tiyenela kutengela . Ana anu amafunika kudziŵa kuti simudzakwiya ndi zimene angakuuzeni . Mwacionekele , io anali atakula kale kuuzimu ngakhale kuti mmishonale uja sanali kudziŵa za masinthidwe amene io anapanga . Manowa anapempha Yehova kuti atumizenso mngelo uja . Iye anati : “ Lolani kuti munthu wa Mulungu woona amene munam’tuma , abwelenso kuti adzatilangize zoyenela kucita ndi mwana amene adzabadweyo . ” — Oweruza 13 : 1 - 8 . ( Ŵelengani Miyambo 15 : 23 . ) Zimene Abulahamu anaphunzila , zinam’cititsa kukonda kwambili Yehova ndi kulimbitsa cikhulupililo cake . Yesu anakamba za anthu 18 amene anafa pangozi pamene nsanja inawagwela , ndipo anaonetsa kuti Mulungu sindiye anacititsa imfa ya anthu amenewo . Yesu anakondwela na mbali iliyonse imene anapatsiwa , nafenso tingacite cimodzi - modzi . 5 : 22 , 23 , 28 , 29 . Ngati wina ali pamavuto tiyenela kucitanji coyamba ? Kucita zimenezi kumalimbitsa ubwenzi wathu ndi iye . — Luka 11 : 9 . [ Mau apansi ] Ife Mboni za Yehova takhala tikupilila pogwila nchito imeneyi m’masiku otsiliza ano cifukwa tili ndi mzimu woyela wa Yehova . Mwadzidzidzi , mahosi akutulukila cothamanga , apo mgugu wa ziboda uli dididi ! Mofananamo , mukamaona zinthu zimene Mulungu analenga , mukamaŵelenga zinthu zimene Yesu ananena zokhudza atate wake , ndi kuganizila mmene Yesu anaonetsela makhalidwe a Atate wake , mudzakhala ndi cithunzi cabwino ca mmene Yehova alili . Mlongoyo anati : “ Ndine wokondwa kwambili kuti mwamuna wangayu anandithandiza kulela mwana wanga . ” Kumbukilani kuti imodzi mwa mfundo zikulu - zikulu mu ulaliki wa Yesu inali yolimbikitsa anthu kulapa macimo awo . 22 : 6 . Mwacitsanzo , tingasinkhesinkhe kukhulupilika kwa Rute . Nthawi zambili , io amasiya ana ao aang’ono kuti azileledwa ndi mnzao wa m’cikwati , mwana wao wamkulu , ambuye ao , acibale kapena anzao . “ Ine [ mtumwi Yohane ] ndinamva mawu ofuula kucokela kumpando wacifumu , akuti : ‘ Taonani ! Ngakhale kuti inu akulu muli ndi maudindo ambili ofunika kusamalidwa mwamsanga , dziŵani kuti kunyalanyaza kuphunzitsa ena kungapangitse kuti mpingo usapite patsogolo . Tinene kuti tikukambitsilana ndi munthu nkhani ya helo . ( b ) N’ciani cikanapangitsa abale a ku Filipi kukhulupilila mau a Paulo ndi kuwaona kukhala ofunika kwambili ? Ngakhale kuti Irina wakhala akukumana ndi mavuto ambili , kukhala wosangalala kumamuthandiza kupilila ndipo amalimbikitsa ena . Mlongo wina , dzina lake Leigh anaona kuti kuganizila funso limeneli kunamuthandiza kucita zinthu mwanzelu . Magazini a m’zinenelo zina anali kufalitsidwa pakapita miyezi ingapo pambuyo pakuti yacingelezi yatulutsidwa . Pamene n’nacoka m’ndende , ananipempha kukalalikila m’matauni osiyanasiyana a m’dziko la kwathu mumzinda wa Kent ndi M’bale Leonard Smith . Ngati tifuna kuti Mulungu azimvela mapemphelo athu , tiyenela kucita zimene amafuna ndi mtima wonse . Paulo anati : “ Cifukwa ca iye tili ndi moyo , timayenda ndipo tilipo . ” Monique na Li Yehova anayankha pemphelo limenelo la Mwana wake wokondedwa , ndipo tsopano anthu mamiliyoni ambili amakhulupilila kuti Yehova anatumiza Mwana wake . 4 : 24 , 30 ; Akol . 1 : 3 ) — 1 / 1 , tsamba 14 . N’cifukwa cake Yehova anayambila kuchula makhalidwe amene amaonetsa kuti iye ni wofunitsitsa kuthandiza atumiki ake . Komabe , Baibulo limakamba kuti kunali anthu okhulupilika monga Yefita ndi mwana wake , komanso Elikana , Hana , ndi Samueli . Pamene Yehova anapempha Aisiraeli kupeleka zopeleka , iye sanakaikile kuti “ aliyense amene anali ndi mtima wofunitsitsa ” adzacilikiza kulambila koona . Tiyeni tiyembekezele . Mwina adzasintha ndi kupulumuka Aramagedo . ” Iye anapatsidwa cisoti cacifumu , ndi kupita kukagonjetsa adani ake ndipo anapambana pa nkhondo yolimbana nao . ” 12 , 13 . ( a ) Kodi Zekariya anauziwa kuti acite ciani ? Tinapemphela kwa Yehova kuti atithandize ndi kutitsogolela popeza tinali pa ulova , tinalibe nyumba , ndipo mwana wathu wacitatu anali ndi caka cimodzi . ( Luka 6 : 35 ) Yesu anali kutsanzila kukoma mtima kwa Mulungu . Pamenepo Filipo anayamba kumufokokozela tanthauzo la zimene anali kuŵelenga . — Machitidwe 8 : 27 - 35 . Komabe , Asa anakumana ndi mavuto cifukwa cocita zinthu mosaganiza bwino . Iye anatilamula kuti tizisonkhana , makamaka pamene mapeto akuyandikila . Motelo , anauza Sara kuti : “ Ndikudziŵa ndithu kuti ndiwe mkazi wokongola m’maonekedwe ako . Ngati mupitiliza kupita patsogolo kuuzimu , mosakayikila Yehova adzakudalitsani . KUSAMALILA ZACILENGEDWE Iye anati : “ N’nayamba kudalila kwambili mnzangayo cakuti nikadabwa ndi mmene anthu anali kucitila zinthu , ninali kupita kukamufunsa ndi kupempha thandizo . Limani minda ndi kudya zipatso zake . ( Aroma 6 : 17 ) Mwacitsanzo , kodi mungacite ciani ngati abwana anu afuna kuti muzigwila nchito kwa maola ambili cakuti mukulephela kupezeka pamisonkhano nthawi zonse ? Ndakonza zimenezi ndipo ndidzazicitadi . ” ( Yes . Koma m’masiku ano otsiliza , tonse timakumana na mayeselo ovuta kuwapilila . Kapena kodi mungawapatse nchito imene angagwile pa nthawi imene abwela kudzaceza m’dziko lawo ? — Mac . 6 , 7 . ( a ) Tisanasankhe zopita ku cikwati cimene cidzacitikila m’chalichi , ndi mfundo zofunika ziti zimene tiyenela kuganizilapo mwakuya ? Allan anakamba kuti , “ M’maŵa tsiku limenelo , mai ameneyo anapempha Yehova kuti a Mboni afike panyumba pake . ” Izi n’zocititsa cidwi cifukwa Mabaibo ambili a Cipangano Catsopano mulibe dzina leni - leni la Mulungu . Koma Baibo imene Hutter anamasulila iye anaikamo dzina la Mulungu . Izi zipeleka umboni woonjezeleka wobwezeletsa dzina la Mulungu m’Malemba Acigiriki Acikhristu . Iwo amayendabe m’kuwala kwa nkhope yanu , inu Yehova . Pemphelo ndi mzimu woyela zidzakuthandizani kusankha mwanzelu , ndipo Yehova adzadalitsa zosankhazo . Conco , cofunika kwambili n’cakuti mnzanu aziona kuti mumam’patsadi ulemu . Zilibe kanthu kaya imwe mumadziona kuti ndimwe aulemu kapena ayi . Şirin , mlongo wa ku Germany , anati : “ Abale a ku Turkey savutika kucita ulaliki wamwayi . Ofalitsa ambili amene apitilizabe kutumikila m’maiko ena mosasamala kanthu za mavutowa apeza madalitso oculuka . — 7 / 15 , tsamba 4 - 5 . 103 : 3 . Baibulo limaonetsa kuti aliyense angathe kukhala bwenzi la Mulungu . Iye anapitiliza kuti : “ Tsiku lina , ndinakumbukila mmene ine ndi mkazi wanga tinali kusangalalila monga banja . Nditakumbukila zimenezi , ndinayamikila Yehova . Panthawiyo , iye analibenso kwina kopita koma kungokhala m’ndende . Pali pano , ciŵelengelo ca ofalitsa caŵilikiza ka 10 kuposa mmene cinalili n’tangofika m’dzikoli . Ngati munthu wina wakamba mau oipa amene atikhumudwitsa , tingacite bwino kukamba naye mokoma mtima . Komabe , Malemba ouzilidwa anakambilatu kuti masiku otsiliza ano , anthu otalikilana ndi Mulungu adzakhala na cikondi cadyela . N’zoonekelatu kuti Petulo anadzicepetsa ndipo analandila uphungu wa Paulo . 11 : 23 - 25 ) Yehova “ anayang’ana ” kuvutika kwa anthu ake , ndipo kupyolela mwa Mose anakonza zowaombola kwa amene anali kuwapondeleza . ( Eks . Mwa kucita zimenezi , timaonetsa kuti ndife odzipeleka pa nyumba ya Yehova monga mmene Yesu anacitila . — Yoh . 2 : 17 . Kodi mufunika kuyamba kusunga zinthu kapena kudzikonzekeletsa mwa kuthupi ? Ngakhale mtumwi Paulo anavomeleza zofooka zake . ( 2 Akor . ( Dan . 4 : 16 ) Yesu anakamba za nthawi imodzimodziyi kuti “ nthawi zoikidwilatu za anthu a mitundu , ” mu ulosi wake wonena za kukhalapo kwake ndi “ mapeto a nthawi ino . ” Ni mafunso ati amene angatithandize kudziŵa mmene tingaseŵenzetsele mfundo ya palembali ? ( Yona 4 : 11 ) Yehova anadziŵa kuti Anineve sanali kudziŵa coonadi ponena za iye , ndipo powamvela cifundo , anatuma Yona kuti akawacenjeze . Njila yaikulu imene anaonetsela cikondi kwa anthu ni mwa kutumiza Yesu kuti adzavutike ndi kutifela . Paulo anagwila mau amenewa , omwe tingawapeze mosavuta pa Aroma 11 : 34 ndi pa 1 Akorinto 2 : 16 . Kodi n’ciani cingathandize posamalila abale ndi alongo okalamba ? M’macaputa onsewa , Mulungu sanam’fotokozela mwacindunji Yobu cifukwa cake anali kuvutika . 12 : 15 ) N’cimodzi - modzinso na akulu . Sayenela kulimbikitsa ndi kutonthoza Akhristu anzawo na mau cabe , koma afunikanso kuwalimbikitsa mwa kuwaonetsa cidwi ceni - ceni . — 1 Akor . “ Mngelo wocokela kumwamba anaonekela kwa iye ndi kumulimbikitsa . ” Mlongo Karen anati : “ Mungapite ku dziko limene kuli ofalitsa Ufumu ocepa kuti mukalaŵe umoyo wa kumeneko . ( Hos . 11 : 4 ; Yoh . Nanga Paulo anawauza ciani pofuna kuthetsa vuto limenelo ? Kodi mumawapewa ndi kuceza kwambili ndi aja amene amafanana ndi inu ? Mwakutelo , Mulungu anapatsa Yesu ulamulilo womenya nkhondo ndi anthu amene amatsutsa ulamulilo wa Mulungu ndi kuwaononga . ( Sal . Yehova yekha ndiye Mulungu wathu . Colinga ca Mulungu cimeneci cinasokonezeka kwa kanthawi pamene Adamu ndi Hava sanamvele Mulungu . ( Gen . Mwacitsanzo , kodi mngelo akanalemba bwinobwino mmene Yona anamvelela pamene anathaŵa nchito yake yopatsidwa ndi Mulungu ? Moyo ni wofunika kwambili kuposa zinthu zakuthupi . Ni zinthu ziti zimene zimapangitsa dipo kukhala mphatso yamtengo wapatali ? Zioneka kuti m’malamulo ao apakamwa aphunzitsi a zipembedzo ena m’nthawi ya Yesu anaikamo mfundo yopezeka pa Ekisodo 21 : 23 , 24 n’colinga cofuna kuvomeleza anthu kubwezela . N’cifukwa cake m’mimba mwanga mukubwadamuka cifukwa ca iye . Mkristu akafuna kupeza lemba , anali kufunikila kutambasula mpukutuwo ndiyeno akamaliza kuŵelenga anali kuupindanso . M’nkhani imeneyi , tidzaphunzila zimene tingacite kuti tipilile citsutso ca m’banja . Kaŵili - kaŵili , Yohane anali kugwila mau a Yesu oonetsa kuti tifunika kuonetsa cikhulupililo nthawi zonse . — Yoh . 3 : 16 ; 6 : 29 , 40 ; 11 : 25 , 26 ; 14 : 1 , 12 . Iye anali kukamba za Akhristu amene anacita zopeleka moloŵa manja kuti athandize pa zosoŵa za okhulupilila anzao . Mbali imeneyi ya masomphenya igogomeza mfundo yakuti Yehova sadzalekelela zoipa zamtundu uliwonse pakati pa anthu ake . “ Sitikufuna kuti mukhale osadziŵa za amene akugona mu imfa , kuti musacite cisoni mofanana ndi mmene onse opanda ciyembekezo amacitila . ” — 1 Atesalonika 4 : 13 . [ Bokosi papeji 6 ] Akufa Adzauka ( Ŵelengani Aefeso 4 : 22 - 24 . ) Mneneli Malaki ananena kuti kumeneku kunali kuyeletsa kwa kuuzimu . Kodi ena amaopa kuceleza alendo pa zifukwa ziti ? Ngakhale n’conco , iye anati : “ Koma ndikufuna mudziŵe kuti mutu wa mwamuna aliyense [ kuphatikizapo memba aliyense wa m’bungwe lolamulila ] ndi Khiristu . . . ndipo mutu wa Khiristu ndiye Mulungu . ” ( 1 Akor . Kodi makolo angathandize bwanji ana awo kuona phindu la mfundo za m’Baibulo ? Mafunso owasinkha - sinkha : 12 : 7 - 11 . CIMWEMWE ANTHU amene amaphunzila Baibulo tingawayekeze ndi ofufuza golide . Ngakhale pa mavuto aakulu , anali kungozisiya m’manja mwa Yehova . Mwininyumba angakhale ndi zocita zina zimene iye amaona kuti n’zofunika . Iwo anasankha kutsatila Satana , mwana wopanduka wauzimu wa Mulungu . Yelekezelani kuti mukuona mmene wodwalayo akuonekela wacisoni pamene Yesu akumufunsa ngati akufuna kucila . Pamene tikukambilana zimene zidzacitika pambuyo pake , tiyenela kukumbukila kuti Mau a Mulungu safotokoza ndondomeko ya mmene zinthu zidzacitikila . Kodi Mose anaonetsa bwanji kuti anali kukhulupilila malonjezo a Mulungu ? TSAMBA 13 • NYIMBO : 65 , 106 Iyo inali kuŵelenga Mau a Mulungu pamene mlaliki Filipo anaifunsa kuti : “ Kodi mukumvetsa zimene mukuŵelengazo ? ” Pambuyo pake , anaphunzitsa Maliko , ndipo anakhala Mkristu wokhwima . Mosasamala kanthu za zimenezi , mwamacenjela Satana anatsutsa zakuti Mulungu ni woyenela kukhazikitsila anthu malamulo m’munda wa Edeni . M’malo mwake , iye anabisa talente yake pansi . Tingacite ciani kuti tizikhulupilila kwambili kuti ulamulilo wa Yehova ndiwo wabwino koposa ? 2 : 17 ) Atate wathu wakumwamba , Yehova , ‘ si wosalungama woti angaiwale nchito yathu ndi cikondi cimene timacisonyeza pa dzina lake . ’ ( Aheb . Kukhala wokhutila ndi wacimwemwe Mulungu anasokoneza cilankhulo ca anthu ndipo anthu amene anali kucilikiza Nimurodi anabalalika “ padziko lonse lapansi . ” Ngati mukuona kuti cifukwa cacikulu n’coti mukutsatila malangizo a m’Baibulo okhudza kukwatiwa “ mwa Ambuye , ” ndiye kuti mukucita bwino cifukwa mukulemekeza lamulo la Mulungu . 22 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi Nkhondo zimene zakhala zikucitika kucokela m’caka ca 1945 ndi za paciweni - weni , koma nazonso ndi zoononga kwambili . Kunyada . Kodi zocita za anthu oipa zimatikhudza bwanji ? KUKHUTILA . Koma msakanizo wamankhwala amene anakonza unali ndi poizoni inayake , ndipo zikuoneka kuti msakanizo monga umenewu ndi umene unamupha . Johannes wa ku Germany anati : “ N’naphunzila zambili zothandiza pa utumiki wanga . Kodi mungakambe naye bwanji ? Kodi Mose anali kuiona bwanji nkhani ya ulemelelo ndi udindo ? ( Luka 4 : 22 ) Tikamakamba mokoma mtima ndi anthu , io angamvetsele zonena zathu ndi kuzikhulupilila . Paulo anakamba kuti : ‘ Kukoma mtima kwakukulu [ kwa Mulungu ] . . . kwatiphunzitsa kukana moyo wosaopa Mulungu ndi zilakolako za dziko , koma kukhala amaganizo abwino , acilungamo ndi odzipeleka kwa Mulungu m’nthawi ino . ’ — Tito 2 : 11 , 12 . Zotulukapo zake zinali zakuti m’masiku ake onse , anthuwo “ sanasiye kutsatila Yehova . ” — 2 Mbiri 34 : 27 , 33 . Gwilitsilani nchito bwino zimene muli nazo . Kuzindikila zimenezi kumathandiza munthu kuti apewe zilakolako zoipa . Kuti izi zitheke , Mboni zinalimbana ndi ndale za mphamvu zacikomyunizimu . Coyamba , pemphani Mulungu kuti akupatseni nzelu na luso la kuzindikila . Nanga n’cifukwa ciani anthu masiku ano akuinyalanyaza ? Iye anati : “ N’nayesetsa kuti nitsilize maphunzilo anga a ku sekondale mofulumilapo ndipo n’nalonjeza Yehova kuti , ‘ Ngati nidzaphasa mayeso , nidzayamba upainiya . ’ ” Mayanjano . Nanga oopsa kwambili ni ati ? ’ Ali na zaka 17 , Eunice anacokadi panyumba , ndipo banja lina la Mboni linam’tenga n’kuyamba kumusunga . N’cifukwa ciani mwina Davide anaona ngati Solomo anali wosayenelela ? Komabe anacita ciani ? Mwacitsanzo , ganizilani za kukula kwa mlengalenga ndi kukongola kwake . 18 : 25 ; Deut . Cinacitika n’ciani ndi cikwati coyamba ? ( b ) N’cifukwa ciani zofalitsa zathu coyamba zimalembedwa m’cingelezi ? ( Chivumbulutso 9 : 1 - 4 ) Yohane anadziŵa kuti dzombe lingaononge zinthu zambili monga mmene linaonongela ku Iguputo m’nthawi ya Mose . Atsogoleli osiyana - siyana amene anapanga zosankha zimene zinayambitsa nkhondo sanadziŵe mavuto amene nkhondoyo idzabweletsa . Koma kodi matendawo anayamba bwanji ? Sitifunanso kuchedwa kuti Revulandi kapena Rabi , kapenanso kuti aliyense azichedwa ndi maina athu eni - eni . ” Paulo analangiza Timoteyo kuti : “ Thawa zilakolako zaunyamata , koma tsatila cilungamo , cikhulupililo , cikondi , ndi mtendele . ” — 2 Tim . Mkati mwa nkhondo yoyamba ya dziko lonse , abale anayesetsa kupeleka cakudya cauzimu na cilimbikitso kwa Ophunzila Baibo amene anali m’malo osiyana - siyana . Popeza kuti Yesu anali Myuda , iye anabadwa ali kale mboni ya Yehova . ( Yes . ( 1 Akorinto 7 : 3 - 5 ) Conco , kukhala mtumiki wa Mulungu sikudalila kuti munthu acite kukhala wosakwatila , ndipo siciyeneletso ca atumiki acikhristu . ( b ) Kodi anthu ena amakhudzidwa bwanji tikakhala oona mtima ? Jairo wakula ndi thanzi lovutikila kwambili . Iye amakondwela ngako akaona kuti tikutengela cifundo cake . 2 : 13 ) Pambuyo pa zaka zambili za mpatuko ndi mdima wa kuuzimu , kodi palinso cina kuposa mzimu woyela cimene cingakwanitse kufotokoza kamvedwe kauzimu kamene kawonjezeleka mwamsanga kuyambila mu 1919 ? Ambili amafunsa kuti : “ Kodi mtumiki wa Yehova angalandile cithandizo ca mankhwala cimeneci ? ” Iye mofunitsitsa wapatula nthawi kuti atithandize kuona mmene tingagwilitsile nchito mfundo za m’Baibulo kuti tibwelele kwa Yehova . Iye anakambanso kuti , “ Kunatithandizanso kukhala ndi nthawi yosangalala ndi malo okongola amene tinali kutumikilako . ” Pelekani citsanzo ca m’Baibo . Koma anakamba kuti ngati Marilyn afuna kupita sadzamuletsa . 65 : 2 ) Kodi inuyo simukuvomeleza kuti lonjezoli ndi lolimbitsa cikhulupililo ? Titakhala zaka zingapo osalankhula Cingelezi , Cituvalu cinakhala ngati cinenelo cathucathu . ( Mateyu 15 : 21 - 26 ; Maliko 7 : 26 ) Kwa Agiriki ndi Aroma , galu inali nyama yokondeka cakuti anali kukhala nayo m’nyumba , ndipo ana anali kuseŵela nayo . Zimene wolandila mphatso amalakalaka . Inde ! Anayankha . Anthu ena amene anali kuŵelenga Baibulo anali kutenthedwa pa mtengo . Akapeza kuti zimene anali kukopela zinali zolakwika penapake , anali kulemba mau ofotokoza zimenezo m’mphepete mwa pepala . Patapita nthawi , nayenso Mfumu Benihadadi wa ku Siriya atadwala , anali kufuna kudziŵa ngati adzacila . — 2 Mafumu 1 : 2 ; 8 : 7 , 8 . Koma buku la Luka limafotokoza kwambili za Mariya , monga za ulendo wake wokaceza kwa Elizabeti , na zimene iye anacita pamene Yesu anatsala ku kacisi . — w17.08 , peji 32 . Florian ndi Anja ndi amodzi mwa amene anatumizidwa kukacita upainiya . Zimenezi zinanithandiza kumakumbukila cifukwa cimene ninayendela kumeneko . Mopanda mantha , iye analankhula ndi Amaziya , wansembe woipa . Zimenezi zionetsa kuti Yehova sanalakwitse kusankha Amosi kuti apeleke uthenga . Atate ao analamulidwa kumanga cingalawa ndi kulowetsamo banja lao lonse . Komanso , “ cisautso cacikulu ” sitingacifulumizitse ngakhale pang’ono . Mukacita zimenezi , mungakhale wotsimikiza kuti Yehova wa makamu adzakutetezani panthawi yonse yotsala m’dongosolo lino la zinthu , komanso mpaka muyaya ! Komanso , musanyalanyaze vuto limenelo ndi kuyembekezela kuti lidzatha palokha . Kodi mapili aŵili amkuwa na magaleta zimatilimbikitsa bwanji ? Pambuyo polimbikitsidwa ndi anthu a zitsanzo zabwino amene tinali kudziŵa , tinadzipeleka kuti ticite ciliconse cimene gulu la Yehova lidzatipempha kucita . N’ciani cidzacitika ? Tsiku limene munthu wabatizika , limakhala nthawi yokondweletsa kwambili . Kuti mudziŵe zambili zokhudza Mboni za Yehova , onelelani vidiyo yakuti Mboni za Yehova — Gulu limene Limalikila Uthenga Wabwino , pa www.jw.org . Ena analeledwa ndi makolo . ( Sal . 32 : 8 ) Koma kuti ubwenzi wathu ndi Yehova ukhale wolimba , tiyenela kukhulupilila kuti iye amamva mapemphelo . Kuti tipewe vuto limeneli , tifunika kumacita zinthu zocilikiza Ufumu nthawi zonse . Ena amakamba kuti Mulungu savomeleza zipembedzo zimenezo cifukwa cakuti siziphunzitsa coonadi . Chris , m’bale amene anayamba kuphunzila Baibulo ndi Gavin , sanakakamize Gavin kuti ayambe kuphunzila Baibulo . [ 2 ] ( ndime 17 ) Onani buku lakuti Jehovah’s Witnesses — Proclaimers of God’s Kingdom , tsamba 662 , ndi bokosi lakuti “ Anafa Cifukwa Copeleka Ulemelelo kwa Mulungu ” limene lili patsamba 150 m’buku lakuti Ufumu wa Mulungu Ukulamulila . Baibulo limatitsimikizila kuti : “ Maso a Yehova ali pa olungama , ndipo makutu ake amamva pembedzelo lao . ” ( 1 Pet . ( b ) Ndi njila yaikulu iti imene Yehova amatikokela kwa iye ? Iwo anamuuza kuti alimbikile komanso kuti azidalila mzimu woyela kuti umuthandize kukhala mutu wa banja wabwino . Iwo mouma mtima , anadya cakudya pafupi ndi citsimeco . 28 : 20 . Izi zikacitika , n’nali kuyesetsa kugwilizana nawo kuti nimvetse bwino cikhalidwe cawo . Kodi Yesu anali kuonetsetsa kuti ali ndi nthawi yocita ciani ngakhale kuti anaika nchito yolalikila pamalo oyamba ? Koma imwe monga kholo , muli na udindo waukulu wom’thandiza mwanayo , maka - maka ngati amakonda kufunsa mafunso . Banjali linakhala kumeneko kufikila Tera atamwalila ali na zaka 205 . Baibo imatiuza kuti ‘ anakhala pansi kudzanja lamanja la mpando wacifumu wa Mulungu . ’ Mngeloyo anakhudza cakudyaco ndi ndodo yake ndipo moto unanyeketsa cakudyaco mozizwitsa . Ataona zimenezi Gidiyoni anazindikila kuti mngeloyo anatumidwadi ndi Yehova . Ngakhale lelo lino , zocitika monga izi zimabweletsa mavuto aakulu m’mipingo ya anthu a Yehova . Kodi mungacite ciani kuti muthetse vuto limenelo ? Zaka mahandiledi zotsatila , pa misonkhano ya chechi komanso anthu ochedwa Azimbo a Chechi , analimbikitsa kusakwatila . 3 : 22 ) Koma zimene munthu amataya akasankha kukhala ku mbali ya Satana , nthawi zonse zimakhala zambili kuposa zimene angapeze kwa Satana . — Yobu 21 : 7 - 17 ; Agal . ( Mat . 24 : 14 ) Pasanapite nthawi , coonadi ca m’Baibo cinayamba kusintha miyoyo yathu . Iye anati : “ Atate anayamba kutaya katundu wosafunika umene tinanyamula m’cola . Conco , Yesu anacenjeza ophunzila ake mwacikondi kuti afunika kupewa ciliconse cimene cikanawalepheletsa kucita zabwino . Kuwonjezela apo , n’nayesetsa kupeza anzanga ena amene n’naona kuti anganithandize kukhala na khalidwe labwino . — Miyambo 13 : 20 . Posacedwapa , Ufumu wa Mulungu udzacotsapo anthu onse amene amatsutsa ulamulilo wa Mulungu . Zipembedzo zonse si zocokela kwa Mulungu woona . Komabe , fanizo la Yesu limatiphunzitsa kuti Yehova amafuna kuti tizikhululuka . Mwacitsanzo , io amatsogolela panchito yolalikila . Kodi zitsanzo za anthu akale amene anacita zinthu molimba mtima zingatipindulitse bwanji ? Kodi izi zitanthauza kuti cikhulupililo ndiye khalidwe lofunika kwambili pa makhalidwe a Akhiristu ? M’zaka zimenezi , tinakondwela na utumiki , tinadalitsidwa , komanso tinali na zokumana nazo zolimbikitsa . ( Genesis 24 : 31 - 33 ) Ganizilani kuti mukumuona akulankhula mwacimwemwe , popeza kuti anali ataona cizindikilo camphamvu cakuti Mulungu wake , Yehova anam’dalitsa paulendo wake wofunika . Kodi tingaonetse bwanji kuti ndise ofatsa ndi odzicepetsa ? 62 : 7 , 8 ; Aheb . 5 : 7 ) Kupyolela m’pemphelo , tingapitilizebe kulankhula ndi Yehova ndi kucita zinthu zom’lemekeza . ( b ) N’ciani cingatithandize kuti tisamacite mantha pocita ulaliki wapoyela ? Iye anauza Yoswa kuti : “ Uza ana a Isiraeli kuti , ‘ Sankhani mizinda yothaŵilako . ’ ” Kodi cilengedwe cimatiphunzitsa ciani ponena za Mulungu ? Mwacitsanzo , pamene Lucia * anamva kuti ku Albania kuli alaliki ocepa , anacoka ku Italy ndi kusamukila kumeneko mu 1993 . Panthawiyo , analibe nchito imene ikanamuthandiza kupeza zofunikila pa umoyo , koma anadalila Yehova na mtima wonse . Kodi ndinu mnyamata kapena mtsikana ndipo mufuna kusankha zimene mudzacita ndi umoyo wanu ? Yesu anati : “ Ndani pakati panu amene mwana wake atamupempha mkate , iye angamupatse mwala ? ( Chivumbulutso 12 : 12 ) Ndiye cifukwa cake iye ndi wokwiya kwambili ndipo akuyambitsa masoka osaneneka pano padziko lapansi . Ngati munthu wina wake watilakwila , tingasankhe kucitapo kanthu kapena kum’khululukila . Yesu anapitiliza kuwauza kuti : “ Mukadzaona magulu ankhondo atazungulila Yerusalemu , mudzadziwe kuti ciwonongeko cake cayandikila . ( Genesis 1 : 31 ) Ndithudi , Mulungu sadzalola kuti dziko lokongolali lionongedwe kothelatu . 24 : 14 ) Ena anacita kupita ku maiko ena kuti akalalikile . Timalimbikitsidwa ndipo timayesetsa kucita zoonjezeleka . Pa nthawi ngati imeneyi , ni cinthu canzelu kukumbukila colinga canu , cimene ni kukwela basi yoyenelela imene ikakufikitseni kumene mufuna kupita . Lemba la Salimo 55 : 22 limati : “ Umutulile Yehova nkhawa zako , Ndipo iye adzakucilikiza . ” Koma pamene anadzidalila , mtima wake unam’nyenga ndipo anacita chimo lalikulu ndi Batiseba . Iye anakonzanso ciwembu cakuti Uriya , mwamuna wa Batiseba , aphedwe . Kodi Yehova amafuna kuti anthu amene samulambila tiziwaona bwanji ? Cisautso cacikulu cidzayamba pamene magulu andale adzaukila zipembedzo zonama , zoimilidwa na hule lochedwa Babulo Wamkulu . ( Chiv . ( Deut . 6 : 4 , 5 ) Ngakhale pamene Farao anaopseza Mose kuti adzamupha , iye sanacite mantha cifukwa anali ndi cikhulupililo , anali kukonda Mulungu , ndiponso anali kuganizila zinthu zabwino zamtsogolo . — Eks . ( 1 Ates . 5 : 12 , 13 ) “ Musafulumile kugwedezeka pa maganizo anu ” ngati mwamvela zinthu zina zofooketsa zokambiwa na anthu ampatuko kapena anthu ena abodza , ngakhale zitamveka ngati zoona . ( 2 Ates . Kodi ndimaŵelenga Baibulo tsiku ndi tsiku ? ( c ) nchito yolalikila ? Nimayamikilabe thandizo limene n’nalandila kwa abale okhwima mwauzimu monga J . ( Kucita zimenezo ndi nzelu . ) Iye anacilikiza Akula mokhulupilika ngakhale pamene zinthu zinasintha . — Mac . 18 : 2 . ( Ŵelengani Yesaya 43 : 1 , 10 , 11 . ) Panthawi imeneyo , mayiyo anayamba kuphunzila Baibo na Mboni ya Yehova . Tikakumana na ciyeso , kukhala na maganizo ofanana ndi a Khristu kudzatithandiza kukaniza ciyesoco . Iye anayang’ananso kwa Yesu ndi kupempha thandizo lake . Pulofesa Susan Rose - Ackerman , amene ndi katswili pankhani yothetsa ziphuphu , analemba kuti “ maboma angafunike kusintha kwambili mmene amacitila zinthu ” kuti akwanitse kuthetsa vuto limeneli . Amayi ake anati : “ Lomba amanitumila foni kapena kunilembela meseji pafupi - fupi tsiku lililonse . COLINGA : Kugwilizanitsa Akristu odzozedwa ndi Kristu kuti akalamulile monga mafumu ndi kutumikila monga ansembe kumwamba Zinthu zimenezi zimaonetsa kuti malo amene Yehova amakhala ndi okongola , osangalatsa ndi amtendele . Ndine wokondwela kwambili kuti pa zaka 30 zapitazi ndathandiza anzanga akunchito 22 kuyamba kulambila Yehova . Pemphelo ndi njila yabwino kwambili ‘ yoyandikila Mulungu . ’ Tingacitenji kuti tipewe malangizo oipa a Satana ? Iwo anaonetsa kuti anali odzipeleka kwa Yehova yekha mwa kukana kudya zakudya zodetsedwa zimene olambila Yehova anayenela kupewa . Yehova watipatsa Baibulo kuti atidziŵitse mmene tingam’tumikilile ndi kum’tamanda . Cifukwa milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi milungu yopanda pake , koma Yehova ndiye anapanga kumwamba . 24 : 22 ) Akristu samatsatila Cilamulo ca Mose , koma tonse timamvela “ cilamulo ca Kristu ” kaya ndife odzozedwa kapena ai . Pali pano , tili ndi ana 9 na adzukulu 11 . Mwa amenewa , 16 akutumikila Yehova ndipo adzukulu athu aang’ono amasonkhana na makolo awo . ▪ “ Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba ” Kenako anati : “ Koma amuna anga mokoma mtima ananithandiza kuona kuti mwana wathu salinso m’manja mwathu , ndi kuti sitifunika kulepheletsa cilango ca Mulungu kugwila bwino nchito . ” Anthu akafuna kum’thandiza , anali kukana . ” Yohane anayamikila Gayo cifukwa coceleza abale ngakhale kuti sanali kuwadziŵa . Nayenso anali ndi nkhawa cifukwa anali kukunkha m’munda mwa munthu amene sanali kum’dziŵa . 3 : 1 - 3 ) Pamene Satana analankhula naye kupitila mwa njoka , Hava anachula lamulo limeneli . Gulaye pomenya nkhondo m’nthawi zakale , 5 / 1 Ndi umoyo wotani umene tikuyembekezela kudzakhala nao m’dziko latsopano ? Zikuoneka kuti anali ndi zaka pafupifupi 20 pamene Yehova anakamba kuti anali olungama mofanana ndi Nowa ndi Yobu . 9 : 10 ) Koma sikuti amenewo ndiwo anali mapeto a zonse kwa iye . Mkulu wa apolisiyo anamuuza kuti : “ Munthu uyu akukana kusaina kuti waleka kukhala wa Mboni . Ni zinthu zina ziti zimene gulu la Yehova likucita masiku ano ? Mungacite bwino kuwafunsa , ndipo mudzalimbikitsidwa ndi mayankho ao . 20 Yehova Amaona Nchito Yanu NYIMBO : 53 , 60 Ndinakula ndi umoyo wokonda mankhwala osokoneza ubongo , njunga , ciwawa , ndi kugwilizana ndi zigaŵenga . Malinga ndi Aheberi 5 : 7 , 11 - 14 , kodi kuphunzila Mau a Mulungu tiyenela kukuona motani ? Tikakhulupilila dipo , timakhala ndi mwayi wokhululukidwa macimo . Kunama nakonso ni mbali ya umunthu wakale . Mwacitsanzo , anthu ambili amakonda kunama pa nkhani za msonkho . M’bale wina ku Germany anacita cidwi kuti buku iliyonse m’Baibulo ili na mfundo zokhudza Ufumu wa Mulungu . N’nali kudziŵa kuti tili paubale wa padziko lonse . Kodi zimenezo zingatheke bwanji ? Zinali zocititsa manyazi kuona kuti mfumu ya Isiraeli ndi asilikali ake , kuphatikizapo abale ake atatu a Davide , akucita mantha . Komanso , acinyamata ambili apindula ndi nkhani zakuti “ Kodi Baibulo Limaphunzitsa Ciani ? ” Anatipempha kuti tikapitilize kutumikila m’dela m’dziko la Nepal . Komabe , iye anadziŵilatu zoipa zimene angadzakumane nazo m’dzikomo . Kodi ndinu wotsimikiza mtima kucita ciani kaamba ka Ufumu ? Ngati muli ndi nthawi , kodi mungandilole kuti ndikuonetseni zitsanzo zingapo zosonyeza kuti mbili ya m’Baibulo ndi yoona ? Iye anayamba kumwa ndi kutukwana monga anzake . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Ciliconse cimene munthu wafesa , adzakololanso comweco . ” — Agalatiya 6 : 7 . Mau a Mulungu anakambilatu za kuuka kwake . Dzifunseni kuti : ‘ Kodi kupeleka moni kuli na ubwino wanji ? YEHOVA anakamba kuti masiku ano , “ amuna 10 ocokela m’zilankhulo zonse za anthu a mitundu ina adzagwila covala ca munthu amene ndi Myuda ndi kunena kuti : ‘ Anthu inu tipita nanu limodzi , cifukwa tamva kuti Mulungu ali ndi inu . ’ ” A Zulu : Palinso ulosi wina wa m’buku la Danieli umene ukunena za Ufumu wa Mulungu . Koma panthawiyo , anali asanapambane nkhondo cifukwa panali patatsala asilikali ena okwana 15,000 a adani . Mogwilizana ndi mfundo ili pamwambayi , Yesu sanalakwitse kuchula amalonda a pakacisi kuti “ acifwamba ” cifukwa anali kudyela anthu masuku pamutu ndiponso anali adyela kwambili . Komanso , Mfumu Sauli ataona kuti Davide zinthu zikumuyendela bwino , anacita nsanje cakuti anafuna kumupha . N’nakondwela kuona kuti M’bale Miller wadzipeleka kupita nane kukakambilana ndi akulu - akulu a bungwelo . Yehova amakwanitsa kucita zimenezi cifukwa cakuti maganizo ake ndi mau ake ndi zapamwamba kwambili kuposa za anthu . Bungwe Lolamulila limagwilizana ndi mau amene mtumwi Paulo analemba kuti : “ Timalankhulanso zinthu zimenezi , osati ndi mau ophunzitsidwa ndi nzelu za anthu , koma ndi mau amene mzimu watiphunzitsa . ” ( 1 Akor . Mmalomwake , anawauza kuti : “ Tangotsimikizani kuti mukati ‘ Inde ’ akhaledi inde , ndipo mukati ‘ Ayi ’ akhaledi ayi . ” — Mat . ( Yoh . 4 : 23 , 24 ) Mwacitsanzo , kuyambila m’caka ca utumiki ca 2003 mpaka 2012 , anthu oposa 2,707,000 , anabatizika kuonetsa kudzipeleka kwao kwa Mulungu . Ganizilani zimene Mulungu anauza Abulahamu kuti acite kwa Isaki , mwana wake wolandila coloŵa amene anamuyembekezela kwa nthawi yaitali . Inde , anasinthadi ndipo amadziimba mlandu akaganizila zoipa zimene anali kucita . Kodi inuyo mumawafikila akulu mukakhala ndi vuto ? Akatswili ena a Baibulo anali atagaŵa Baibulo m’njila zosiyanasiyana . Makhalidwe amene anachula ni ofanana ndi amene ali pa Aroma 1 : 29 - 31 . Conco , njila imodzi imene ‘ mungakumbukile amene akutsogolela ’ ndi mwa kuchula Bungwe Lolamulila m’mapemphelo anu . Sikudzakhalanso madokota kapena mankhwala . Tingakhulupilile kuti zimene Baibo imakamba n’zoona . Erica anakamba kuti , “ ukathandiza munthu kudziŵa Yehova umapeza cimwemwe cosaneneka . ” Ndipo pakati pa anthu amene anathandiza kumanganso mpandawo panali ana a Salumu , kalonga wa hafu ya cigawo ca Yerusalemu . ( Neh . Mboni zimenezo zinafotokoza kuti pa cifukwa cimeneco , izo sizikhulupilila Utatu . Monga mmene Nowa anapulumukila Cigumula , Akhristu okhulupilika obatizika adzapulumuka pamene dziko loipali lidzawonongedwa . ( Maliko 13 : 10 ; Chiv . Ulosiwu ukuphatikizapo “ ufumu wa anthu , ” umene ndi ulamulilo wa Mulungu pa anthu . Panthawi zonse ziŵili , iye anapha zilombo zolusazo . — 1 Samueli 17 : 34 - 36 ; Yesaya 31 : 4 . 3 : 4 ) Kufotokoza mwa njila imeneyi n’kwabwino ndipo n’kofika pamtima . Nthawi zambili , anali kunilola . Koma sunali kukhala ulendo wabwino kweni - kweni . Mwacitsanzo , munthu akakhala ndi mnzake , ubwenzi wao umakula pang’onopang’ono . * Mwambi wa anthu a pa cilumba umati : ‘ Civomezi camphamvu cikayamba pa nyanja ndipo madzi akayamba kuoneka monga akucepa , thaŵilani ku mapili cifukwa madzi akakhutukila kumtunda adzaloŵa m’nyumba . ’ Kwandithandizanso kukhala mwamuna komanso tate wabwino . ( Mat . 4 : 17 ) Koma panthawiyi , Yesu anazindikila kuti ena mwa ‘ okhometsa msonkho na anthu ocimwa ’ anali kufuna kusintha . ZIMENE MAU A MULUNGU AMAPHUNZITSA : Mulungu wapeleka kale njila yabwino koposa pofuna kuthandiza ndi kulimbikitsa anthu . Conco Davide anakonzekela kuti akalange Nabala cifukwa comuyankha mwamwano ndi kucita zinthu mosam’ganizila . 6 : 16 ; Chiv . Cinsinsi cake cagona pa kum’dziŵa molondola Mulungu . Mulungu anadzoza Yesu ndi “ mafuta acikondwelelo cacikulu ” kuposa “ ca mafumu ena , ” kutanthauza mafumu aciyuda omwe anali mu mzela wa Davide . Pankhani yokhudza cithandizo ca mankhwala , aliyense afunika kusankha yekha , ndipo ayenela kuvomeleza zotsatilapo za zosankhazo . Umboni wotani ? Demetrius na Mboni zina pa cisumbu ca Makrónisos Mfumu imeneyi yakwela pahachi “ cifukwa ca coonadi , kudzicepetsa ndi cilungamo . ” 3 : 21 ) Yehova amayankha pempho lathu limeneli mwa kutiyeletsa na magazi a nsembe ya Khiristu . Ndipo ucimo unamugonjetsa . Ndinasangalala kuona kuti Amai , Atate , ndi acibale anga ena anabwela ku phwando la cikwati cathu . Zimenezi ziyenela kuti zinayesa cikhulupililo ca acibale a Naboti ndi mabwenzi ake . 4 : 17 - 21 ) Apa Aisiraeli anagonjetsa adani awo kothelatu . 12 , 13 . ( a ) N’cifukwa ciani tifunika kucita zinthu zonse moona mtima ? Kukhululukilana kumathandiza kuti banja likhale lolimba ndiponso kuti muyandikilane kwambili . ” Mneneli Yesaya anauzilidwa kulemba za ciitano cosangalatsa cimene cikupelekedwa “ m’masiku otsiliza ” ano . Ciitano cimeneci cikuti : “ Bwelani anthu inu . Kuwala kwa Coonadi Kufika m’Dziko la Japan , 11 / 15 Onse akali kutumikila Yehova mokhulupilika . Ni zinthu zina ziti zimene anthu amafuna ? Buku yakuti Celibacy and Religious Traditions , inakamba kuti mwambo umenewu “ wopewa za kugonana unali m’citidwe watsopano umene unayambika mu Ufumu wa Roma . ” Chechi na Boma zinalimbikitsa Cikhristu campatuko ndi kupondeleza Akhristu amene anali monga tiligu . Ndiponso Atate wathu wakumwamba amene ndi wacikondi amatamandidwa . Anthu padziko lonse amaganizila mafunso ofunika kwambili . Aisiraeli a m’nthawi yakale anali citsanzo cabwino ca dongosolo la Mulungu . 1 , 2 . ( a ) Ni vuto lanji limene makolo amakhala nalo ? Nanga angacitepo ciani ? Iye anali ndi mwayi wophunzila Baibulo . ( Ŵelengani 2 Timoteyo 3 : 12 . ) ( b ) Kodi n’ciani cinapangitsa ‘ mau otuluka m’kamwa mwa Mfumu kukhala osangalatsa ’ ? Ndipo ife tingatengele bwanji citsanzo cake ? Timaonedwa olungama pamaso pa Mulungu . Cidwi cimene anadzutsa paulendo woyamba , mwacionekele n’cimene cinacititsa kuti pa maulendo ake otsatila , anthu mahandiledi , ndipo nthawi zina masausande , azibwela kudzamvetsela nkhani zake . Koma kodi ndinu okhutila ndi mayankho anu ? N’cifukwa ciani kugonjela mwacikondi n’kofunika ? Iwo ni aciyambakale ndiponso ni akatswili pa nkhondoyi . Ndipo anthuwa anatsala ku Yerusalemu kwa kanthawi kuti alimbikitsidwe mwa kuuzimu . ( Yakobo 4 : 8 ) Baibulo limatitsimikizila kuti : “ Yehova ali pafupi ndi onse oitanila pa iye . ” ( b ) Kodi Dema anaonetsa bwanji kuti anali kukonda zinthu za m’dziko ? Muzipeleka citsanzo cabwino pa zokamba ndi zocita zanu . Iwo anatipatsa mbali pa kuŵelenga Baibulo kwa mlungu ndi mlungu , ndipo tinali kukonza mafunso ndi mayankho ophunzila pa misonkhano imene abale anakonza . Iwo samadzisankhila okha zovala zimene ayenela kuvala , koma ena ndi amene amawasankhila . ” — Adrian . Nanga kodi Akristu ayenela kupita ku tuakacisi kukalambila ? Olo tikumane na mavuto otani , tiyeni tiziika cifunilo ca Yehova patsogolo mu umoyo wathu , ndiponso tizimudalila na kumumvela na mtima wonse . Kucita zimenezi kudzakuthandizani kuti musadzakhale mbali ya dzikoli pamene lidzaonongedwa . MBILI YA BANJA LALIKULU Yosefe anali kucokela ku banja lalikulu , limene linali losagwilizano ndi losasangalala . Tikamba pano , padziko lonse pali Nyumba za Ufumu pafupi - fupi 2,500 zimene zikumangiwa kapena kukonzewanso . Panafunika khama kuti anivomele , ndipo zinatheka . Kodi tingaonetse m’njila ziti kuti ndise acifundo ndi okoma mtima ? Ndipo izi zimanilimbikitsa kugwila nchito yolalikila . ” ( Aroma 12 : 1 ) Pa zifukwa zimenezi , opita ku ubatizo amafunsidwa mafunso kuti avomeleze ngati anadzipelekadi kwa Yehova kuti acite cifunilo cake . Mwacionekele , zimene taphunzila zatithandiza kuyamikila kwambili buku louzilidwa limeneli la m’Baibulo . Kodi Akristu ayenela kuwaona bwanji maulendo opita kukalambila ku tuakacisi ? N’zocititsa cidwi kuti Inoki anakhala na moyo zaka 365 . 13 Amuna a Paudindo — Tengelani Citsanzo ca Timoteyo Anthu ena amakamba kuti Baraki analibe cikhulupililo cifukwa ca kupempha Debora kuti apitile naye limodzi , koma zimenezo sizoona . Enanso ambili amayamikila akalandila Baibo na zofalitsa za m’citundu cawo , akalandila thandizo pa nthawi ya tsoka la zacilengedwe , kapena akaona zotulukapo zabwino za ulaliki wa pa tumasitandi ndi wapoyela m’dela lawo . Cacikulu koposa amatiuza zimene tingacite kuti tikapulumuke . M’nkhani ina , ndinaŵelenga za mai wina amene analimbikitsa mwana wake wamkazi kuti Yehova adzam’samalila mwa kumuuza kuti , ‘ Yehova angakusamalile bwino kuposa ine . ’ Zingakhalenso bwino kusonkhana ndi abale ndi alongo akumeneko ndi kupita nao mu ulaliki . Kenneth anati : “ Tikusangalala kwambili , osati cifukwa cakuti tilibe mavuto , koma cifukwa cakuti tili ndi umoyo wopindulitsa . 84 : 10 ) Izi n’zosadabwitsa cifukwa , monga Mlengi wathu wacikondi , Yehova amadziŵa bwino zimene timafunikila kuti tikhale na cimwemwe ceni - ceni , ndipo amatipatsa zonse zofunikila . N’ciani cingakuthandizeni kuti musavutike kuyamba kuŵelenga Baibo ndi kuti muzisangalala pamene muŵelenga ? Iye anati : “ Kukambilana nkhani za conco kwathandiza kuti anthu atidziŵe ndi kulandila zofalitsa zathu . Popeza nthawi zina mauthenga amenewa sitingawazindikile , katswili wina wa cikhalidwe ca anthu , dzina lake Vance Packard , anati : “ Ambili a ise timasoceletsedwa kwambili , koma osadziŵa . ” Koma Yesu anamuyankha mwamphamvu kuti : “ Pita kumbuyo kwanga , Satana ! ” ( Mat . N’kutheka kuti anagwila nchitoyi kwa zaka zoposa 1,600 mpaka panthawi ya Cigumula . Mtumwi Petulo anauzilidwa kulemba kuti : “ Conco popeza zinthu zonsezi zidzasungunuka , ganizilani za mtundu wa munthu amene muyenela kukhala . Muyenela kukhala anthu akhalidwe loyela ndipo muzicita nchito zosonyeza kuti ndinu odzipeleka kwa Mulungu . ( 2 Akorinto 11 : 24 - 27 ) Panthawi ina , Timoteyo anaikidwa m’ndende cifukwa ca cikhulupililo cake . Nkhondo itatha , kunabukanso mavuto a njala ndi umphawi wadzaoneni . Ambili a io amafika pamisonkhano ndipo mmodzi amatumikila nafe monga mpainiya . ” Anthu amene ali m’gulu la okana Kristu amadzicha kuti ndiwo Kristu kapena omuimila . Koma mufunika kulandila thandizo limene amapeleka kupitilia mu mpingo wake . ( Miy . 24 : 16 ; Yak . Ni mavuto anji amene Nowa anakumana nawo pomanga cingalawa ? Ngati munthu wina watikhumudwitsa mwadala , tisalole kukhala ziwiya za Satana zosungilamo mkwiyo . Tifunika kukumbukila kuti dziko loipali na zonse za m’dziko n’zosagwilizana ndi cifunilo ca Yehova kapena maganizo ake . ( Yak . Nanga zimenezo zingatheke bwanji ? ” Tikanangomudziŵa kuti ndi munthu amene anapanga cingalawa ndi kupulumutsa banja lake ndi nyama . Kodi tingathandize bwanji abale a Kristu mokhulupilika ? Nanga n’cifukwa ciani ino ndiyo nthawi yocita zimenezi ? Nanga zinacitika bwanji kuti tikhale ndi adani ambili amene amatilanda cimwemwe , monga mdani wathu wamkulu amene ndi imfa ? Tinayankhanso kuti , “ Nanga bwanji ngati mmodzi wa asilikali waona kuti tili na hachi , ndipo watilamula kuti tinyamule zida n’kukapeleka kwa omenya nkhondo ? ” Anatenga Samueli n’kupita naye kwa Mkulu wa Ansembe Eli , ku cihema ku Silo . Mboni za Yehova za m’dela lanu n’zokonzeka kukuthandizani kumvetsetsa Baibulo , ndi mmene mungaseŵenzetsele mfundo zake . TSAMBA 15 KODI PALI ZIMENE MUNGACITE NA MMENE MOYO WANU UDZAKHALILA M’TSOGOLO ? Iye anakamba kuti ulamulilo wa Mulungu ni woipa ndi kuti Yehova amamana zabwino anthu ake . 2 : 17 ) Ndiyang’ananso mtsogolo kudzaona anthu akuukitsidwa padziko ndili kumwamba , ndi kudzaonanso atate wanga a kuthupi . Hans Hölterhoff anali kuseŵenzetsa ngolo iyi polengeza za The Golden Age ( imene tsopano imachedwa Galamukani ! ) mu ulaliki ? Mtumwi Paulo anakamba kuti munthu wakuthupi sangathe kuzindikila kulakwa kwake pa maso pa Mulungu . Kodi Adamu analephela bwanji kuseŵenzetsa bwino ufulu wake ? Timadziŵa bwanji kuti amuna ndi akazi okhulupilika ochulidwa m’Baibulo anali kuganizila za mphoto yao ? Ndipo anakwanitsa bwanji kucita zimenezi ? Kodi ophunzila a Yesu anakwanitsa kucitila umboni za iye molimba mtima ? Musaiŵale kuti Yesu anatumiza ophunzila ake “ aŵiliaŵili ” kokalalikila . Yosefe sanali kudziŵa kuti zimene amuna amenewo adzamufotokozela zidzasintha kwambili umoyo wake . Kodi Yesu analankhula bwanji mwacifundo kwa ena . ( a ) N’cifukwa ciani nchito yolalikila tiyenela kuiona kukhala yofunika kwambili mu umoyo wathu ? Kodi Nkhani Zimene Zili M’Baibulo Ndi Nzelu za Anthu ? Kuyambila ali mwana , Jairo wakhala ndi thupi lofooka ndipo amadzidzimuka . Ngakhale ndi conco , ali ndi ciyembekezo colimba ca tsogolo labwino . Kuonjezela apo , Yehova anakamba kuti cifunilo cake sicisintha . Tingaonetse bwanji mzimu woceleza kwa alendo odzakamba nkhani mu mpingo mwathu na alendo ena oimilako gulu la Yehova ? Conco , pamene Luka anachula Yosefe ndi kunena kuti anali mwana wa Heli , anthu anadziŵa kuti anali kutanthauza kuti Yosefeyo anali mkamwini wa Heli . — Luka 3 : 23 . Ngakhale kuti kuukapolo kuja Ayuda anali kupeza zosoŵa zawo zakuthupi , nanga bwanji zinthu zauzimu ? Kodi nimayesetsa kulimbitsa ubwenzi wanga na Mulungu ? ’ 1 : 8 , 9 , 13 , 14 . Yesu amene ndi Mkwati , adzabwela kudzapeleka ciweluzo cisautso cacikulu cikatsala pang’ono kutha . Mwina iye angaganize kuti , ‘ Ndilibe nthawi yosintha oilo , ndipo ngakhale ndisaisinthe , galimotoyi ipitilizabe kuyenda kwa kanthawi . ’ Mungayambe kudzifunsa kuti : ‘ N’cifukwa ciani zimandivuta kusintha zinthu zing’onozing’ono zimenezi ? Mofanana ndi Abulahamu , mtumwi Paulo na mnzake Sila nawonso anali kuganizila kwambili za malonjezo a Mulungu . ( Sal . 15 : 1 ) Davide anayankha funsoli mwa kuchula makhalidwe abwino amene Mulungu amafuna kuti alendo ake akhale nawo . Mwamuna wina wochuka pakucilikiza mgwilizano wa zipembedzo wochedwa Dalai Lama anati : “ Miyambo yonse ya zipembedzo imacilikiza cikondi , cifundo ndi kukhululukilana . Tikatelo , tidzalimbikitsa mgwilizano m’gulu lathu , limene ni banja la alambili a Yehova . N’cifukwa ciani Paulo anapulumutsidwa “ mkamwa mwa mkango ” ? ( b ) Ni fanizo lanji limene Yakobo anakamba pofotokoza za kuleza mtima ? Lamulo limene anakhazikitsa pankhaniyi , lionetsa kuti khalidwe loipali linali kucitika kaŵili - kaŵili . ” Yesu anapemphela kwa Atate wake “ ndipo anamumvela . ” — Aheberi 5 : 7 Ŵelengani Mateyu 6 : 34 . Pa cifukwa ici , Yehova analola Mfumu Sisaki ya Iguputo kulanda mizinda yambili ya Yuda , olo kuti Rehobowamu anali atailimbitsa kwambili . — 1 Maf . Kumvela Cenjezo , Na . Kaya mumagwila nchito ya muofesi , yamanja , kapena nchito zina , dziŵani kuti “ kugwila nchito iliyonse kumapindulitsa . ” Pa nkhani zina , Akhristu angapange zosankha zosiyana olo kuti onse ali na zikumbumtima zophunzitsidwa bwino Baibo . Anthu amene ali mu utumiki wanthawi zonse anasankha nchito yokondweletsa ndi yopindulitsa kwambili . Kuti tipeze yankho , tiyeni tipendenso nkhani ya Paulo na Sila . Ndiyeno mwamunayo anafunsa Rabeka kuti : “ Kodi ndiwe mwana wa ndani ? Ngati ana ali na makhalidwe abwino , kholo losakhulupilila lingakopeke n’kuyamba kulambila Mulungu . Conco , pemphani thandizo kwa anthu amene amaŵelenga Baibo ndi maganizo odzicepetsa , amene amadalila mzimu wa Mulungu kuti aimvetsetse , komanso amene amakhulupilila kuti tili m’nthawi imene Mulungu afuna kuti anthu amvetsetse Baibo . A Daka : Nanga n’cifukwa ciani anthu amanena kuti simukhulupilila Yesu ? Yehova sanacite zimenezo , koma analola Satana kuyesa Yobu . N’cifukwa ciani kukhululukilana n’kofunika ? Nanga n’cifukwa ciani anthu amapemphela ? Baibo imakamba kuti ngakhale ‘ tsitsi lenilenilo la m’mutu mwathu amaliŵelenga . ’ ( Mat . Mpainiya wanthawi zonse alalikila mzimayi wamalonda m’citundu ca Cikwichuwa ( Imbabura ) , pa msika wogulitsila nsalu mumzinda wa Otavalo , kumpoto kwa dziko la Ecuador . KUPHANA : Zioneka kuti anthu pafupifupi 500,000 amene anaphedwa m’caka ca 2012 , anali oculuka kuposa amene anafa pa nkhondo . Yehova anatuma moto kucoka kumwamba kuti unyeketse Nadabu ndi Abihu , ana a Aroni . 4 : 20 , 21 ; Sal . Mapale amenewo anawapeza mu 2012 . Nanga n’cifukwa ciani Akristu masiku ano afunika kuyembekezelabe ? * Nduna imeneyi inalandila thandizo kucokela kwa wophunzila wa Yesu , dzina lake Filipo , amene anali mphunzitsi wofikapo wa Mau a Mulungu . Mwamuna wanga anamwalila ndipo sindikwanitsa kucita zonse zimene ndinali kucita kale . Mafumu ndi olamulila a m’zaka za m’ma 1500 anali kuchula adani ao kuti okana Kristu . ( Ŵelengani Yohane 2 : 3 , 6 - 11 . ) Kucita zimenezi sinali nkhani yamaseŵela . Pamene Yesu anauza otsatila ake kuti azikhululukila ngakhale amene amawalakwila mobwelezabweleza , io anam’pempha kuti : “ Tionjezeleni cikhulupililo . ” — Luka 17 : 1 - 5 . Kaya mukumana na mavuto abwanji , mungathe kupeza citonthozo . Iye anati : “ Ndinacotsedwa pa nchito ya zomangamanga imene inali ya malipilo abwino . ” Kodi pali aliyense amene anandiuzapo kuti ndisiye kum’tumila mauthenga ? ’ ( Yes . 61 : 1 ) Iye anaitana onse “ ogwila nchito yolemetsa ndi olemedwa ” kupita kwa iye kuti ‘ akatsitsimulidwe . ’ ( Mat . 94,101 Kodi imfa ya Yesu inapatsa anthu mwai wotani ? Ndimaona kuti ana anga anakwatila akazi auzimu amene amakonda Yehova Mulungu ndi mtima wao wonse ndiponso moyo wao wonse . — Aef . Ngati anthu amene nimaphunzila nawo Baibo kapena amene nimacitako maulendo obwelelako aonako zosangalatsa zanga , kodi angaone kuti nimacitadi zimene nimawaphunzitsa ? ’ Nanga ndi zinthu ziti zimene akulu ayenela kucita kuti akwanitse kuphunzitsa ena ? Iwo anali kupenda mau ndi zilembo mosamala kuti pasapezeke zolakwika zilizonse . Iye anati : “ N’nali kuwanyalanyaza ndi kuwapewa . N’nakhalanso wosangalala ndi wokhutila . ” Iye anakwatila mlongo wokamba Cizungu . Zinthu zodetsa . M’nkhani ziŵilizi , tidzakambilana mmene Yehova amaonetsela cikondi cake pa ife ndi mmene tingaonetsele kuti timam’konda . Shan , amene ndi mkulu mumpingo , anati : “ Amayi sanali kumvetsetsa citundu cimene ife tinali kudziŵa , ndipo ine na azilongosi anga tinali kulephela kukamba bwino citundu cawo . Umboni Winanso ( Tatenai analikodi ) , Na . Komabe , nthawi zina timafunika kuganizilaponso pa cosankha cathu . Kodi zinali zomveka kuti Davide ayembekezele Mulungu kumuŵelengela ? Komabe , ngakhale anthu amene samvetsela uthenga wathu amatilemekeza cifukwa ca nchito imeneyi . ( Mat . 24 : 42 - 44 ) Koma tiyenela kukhala oleza mtima ndi achelu nthawi zonse . ( The Columbia History of the World ) M’malo mothetsa cidani , atsogoleli acipembedzo anasonkhezela cidani . Mpaka pano zilembozi n’zacinsinsi m’lingalilo lakuti zithunzi zake sizinapezekebe . 6 : 9 , 10 ; Chiv . Mwana amayamba kukhwima m’maganizo mwa kuona zimene makolo ake amacita na kutengela citsanzo cawo cabwino . Lomba sinicita manyazi kwambili ngati mmene n’nali kucitila poyamba . ” Coyamba , Paulo anakumbutsa magulu onse aŵili kuti cakudya sicingawapezetse ciyanjo ca Mulungu . Pamene Ayuda anali kuyenda , nthawi zambili ayenela kuti anali kuganizila za Yerusalemu , malo awo atsopano okhala . N’cifukwa cakuti iye ndi Atate ake saloŵelela m’mikangano ya m’dzikoli . Nanga kuona “ Wosaonekayo ” kunam’thandiza bwanji pamene iye ndi anthu ake anali pa mavuto aakulu ? SANAOPE MFUMU Zimenezi zikapitiliza kucitika , mkupita kwa nthawi , ubwenzi wathu ndi Yehova umalimba . Yesu anamveketsa bwino mfundoyi pamene Mfarisi wina anam’funsa kuti : “ Mphunzitsi , kodi lamulo lalikulu kwambili m’Cilamulo ndi liti ? ” Koma tifuna kukutsimikizilani kuti n’zotheka Akristu oona kupewa ciwelewele mwa kuthandizidwa ndi Yehova . — Ŵelengani 1 Atesalonika 4 : 3 - 5 . Kodi pemphelo lathu lakuti “ Ufumu wanu ubwele ” lidzayankhidwa liti kothelatu ? Ngati zili conco , Mkristu afunika kuyesetsa kulimbitsa cikwati cake mwa kupitilizabe kumvela malangizo a m’Baibulo . ( 2 Mbiri 20 : 17 ) Koma kumwamba kudzacitika zinthu zosiyanako . ( Salimo 84 : 1 - 3 ) Kodi ife pamodzi ndi ana athu timalaka - laka kuti nthawi zonse tizisonkhana pamodzi na anthu a Mulungu monga anacitila wamasalimo ? — Salimo 26 : 8 , 12 . Tikaganizila zimene zakhala zikucitika zaka zaposacedwapa , timaona mmene Mulungu amasamalilila anthu ake . M’baleyu anakamba kuti anthu amamasuka akadziŵa cifuno cowacezela . 4 : 4 ) Satana Mdyelekezi alinso ndi “ njila yobweletsela imfa . ” Nakhala Zinthu Zonse Kwa Anthu Osiyana - siyana ( D . Koma panthawiyi , ananyamula zida zoopsa za nkhondo . Iye anali wamphamvu kwambili ndiponso wodziŵa kumenya nkhondo . Anthu ambili anamva uthenga wabwino . Wendy ( Gen . 3 : 16 - 19 ; Aroma 5 : 12 ) Pamene anthu oyamba anacimwa , padziko lapansi panalibe amene anali kugonjela Mulungu . Dziko lapansi lidzasintha kukhala paradaiso . — Yesaya 35 : 1 , 6 . Mulungu adzathetselatu vuto lokoka fodya , ndipo adzacititsa anthu kukhala ndi matupi ndi maganizo angwilo . — Yesaya 33 : 24 ; Chivumbulutso 19 : 11 , 15 . Nanga zimenezo zimakhala ndi zotsatilapo zotani ? Pali “ zinthu zambili zodabwitsa ” zimene ‘ sitingathe kuzifotokoza zomwe Yehova amaticitila . Palibe amene adziŵa NYIMBO : 81 , 70 Kodi timaonetsa bwanji kuti tikumvela “ cilamulo ca Kristu ” 12 : 25 . Koma cacikulu n’cakuti tifunika kuwathandiza kuti azigwilizana ngako na mpingo wawo watsopano . MWAMUNA wina amene wakhala m’banja lacimwemwe kwa zaka 38 anati : “ Ngati mumacita khama kuti banja lanu likhale lolimba , Yehova adzakudalitsani . ” Kenako anati , “ Ngati winawake anakupatsani bukuli , mundipatse kapena mulitaye ! ” Conco , pamene Yesu anauza atumwi ake kuti : “ M’nyumba ya Atate wanga muli malo ambili okhalamo , ” anali kukamba zinthu zimene anadzionela yekha . — Yohane 6 : 38 ; 14 : 2 . Mwacitsanzo , ngati ndinu wacinyamata , mwina mumamva anzanu a kusukulu akudzitama kuti amagonana ndi anthu osiyanasiyana kapena kutumizilana zithunzi ndi mauthenga okhudza kugonana . Conco , pamene Yesu anali kudya cakudya pamodzi na atumwi ake pa tsiku lakuti iye adzaphedwa maŵa , anawauza kuti atenge malupanga aŵili . Njila imodzi yaikulu imene Satana amanyengela anthu ndi kupitila m’cipembedzo conama . Cilengezo citapelekedwa , anthu odzipeleka anasonkhana pa Phili la Tabori . Pa cifukwa cimeneci , ndinalembela kalata ofesi ya nthambi ya Mboni za Yehova . Lemba la Mateyu 7 : 24 - 27 , limafotokoza fanizo la Yesu lokamba za amuna aŵili amene aliyense anamanga nyumba yake . 24 : 45 , 46 . Nanga tingakhale bwanji odzicepetsa pamene zinthu n’zovuta , kapena pamene athu ena atisoŵetsa mtendele ? ‘ Zimenezo Uziphunzitse kwa Amuna Okhulupilika , ’ Jan . Posakhalitsa , n’nakumana na m’bale Walter Bright , amene analoŵa kilasi ya namba 30 ya Giliyadi . Pambuyo pokambilana ndi akulu - akulu a bungwelo , m’caka comweco ca 1954 anavomeleza kuniona monga mtumiki wa Mulungu . Kodi ndani kwenikweni akulamulila dzikoli ? Koma tinasankha kuika maganizo athu pa nchito yatsopano monga mmene amayi akanafunila . Kukamba kwina tingati n’nali kudziphunzitsa nekha coyamba n’colinga cakuti nikaphunzitse wophunzila wanga . * Apa , Yesu sanali kulimbikitsa ophunzila ake kuti azicita zacinyengo n’colinga cakuti apeze zofunikila pa umoyo wawo . Koma zimenezi zikacitika , n’nali kupita kwa amene anali kuniphunzitsa Baibulo kuti anilimbikitse ndi kunithandiza . Anthu ambili amakonda sopo wanga ndipo amauzako ena . NYIMBO : 80 , 50 Anthu ambili saupeza mtendele wa maganizo . ( Salimo 37 : 10 , 11 ) Koma mwina mungafunse kuti : ‘ Kodi Mulungu amangolanga anthu osawacitila cifundo ? ’ Mlongo wina anakamba kuti anali kucita mantha kuyankhapo pa phunzilo la Nsanja ya Mlonda . 1 , 2 . ( a ) Kodi Elifazi ndi Bilidadi anakamba kuti Mulungu amauona bwanji utumiki wathu ? ( Mateyu 23 : 8 ) Cacitatu , kumbukilani kuti Yesu anati : “ Zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inunso muwacitile zomwezo . ” N’zolimbikitsa ngako kuona abale ambili oikidwa kumene pa udindo , monga imwe , akuyesetsa kupita patsogolo mwauzimu . ( Mateyu 28 : 19 , 20 ) Conco , monga otsatila a Yesu , tifunika kucita zinthu zinai izi : Tiyenela kupanga ophunzila , kuwaphunzitsa , ndi kuwabatiza . Mau a Yesu a pa Yohane 5 : 22 , 23 amamveketsa bwino mfundo imeneyi . Iye anati : “ Atate saweluza munthu aliyense , koma wapeleka udindo wonse woweluza kwa Mwana , kuti onse alemekeze Mwana monga mmene amalemekezela Atate . Kungalepheletse mzimu woyela kugwila nchito bwino mumpingo . Tidzalandila anthu amene adzaukitsidwa ndi kuwaphunzitsa za Yehova . Cifukwa cake n’cakuti , mofanana ndi Yesu , ifenso tinalengedwa m’cifanizilo ca Mulungu . Ndipo ngakhale Danieli iye mwini sanamvetsetse zimene analemba . Olo kuti sukulu n’nalekezela giledi 7 , n’nakwanitsa kucita izi cifukwa nthawi zambili matica athu anali kuseŵenzetsa Cizungu pophunzitsa . Mwacitsanzo , Paulo analemba kuti abale ena ku Roma anali akapolo a “ mimba zawo [ kapena zilakolako zawo ] . ” Izi zitanthauza kuti iwo anaika patsogolo zakugonana , kudya , ndi zinthu zina . Ndiyeno , Mulungu adzapatsa anthu onse omvela mtendele ndi zinthu zambili kuti adzasangalale ndi umoyo . ( Sal . 5 : 1 , 2 . ( Gen . 3 : 6 ) Komanso , ganizilani za mavuto ambili - mbili amene anthu akumana nawo kucokela nthawi ya Adamu cifukwa colephela kukhala odziletsa . 2 FUNSO : Kodi Yesu n’ndani ? Mofanana ndi Akhristu a ku Galatiya amene Paulo anawalembela kalata , na ise tifunika kupewa kukhala akapolo a zinthu “ zacibwanabwana , zomwe ndi zosathandiza ndiponso zopanda pake ” za m’dzikoli . Ngati n’conco , ndiye kuti muphunzila zambili pa cikhulupililo cimene Inoki anali naco . Akhiristu atsopano onsewo anakhala “ fuko losankhidwa mwapadela , ansembe acifumu , mtundu woyela , anthu odzakhala cuma capadela . ” Pambuyo pake , anabwelela ku Yerusalemu . Koma akakhala na nkhawa kwambili , anali kupemphela kaŵili - kaŵili , kupempha Yehova kuti amuthandize . Kusindikizidwa kwa zofalitsa m’zinenelo zosiyanasiyana , kwathandiza kuti anthu aphunzile Baibulo m’cinenelo cimene afuna . M’BALE Guy Hollis Pierce , amene anali membala wa Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova anamaliza moyo wake wa padziko lapansi pa Ciŵili , March 18 , 2014 . Mwacitsanzo , akatswili ena amakaikila ngati zimene zili m’Mabaibulo a masiku ano n’zimenenso zinali m’mipukutu yoyambilila ya Baibulo . Zambili mwa nyimbo za m’buku lakuti ‘ Imbani Mokweza ndi Mosangalala ’ kwa Yehova , ’ zili monga mapemphelo . N’nayamba kudzimvela cisoni kwambili . Koma n’nali kupita ku midzi imene anali kukhala , kukawalimbikitsa kuphunzila Baibo . 1 : 3 ) Conco , kukulitsa cikhulupililo cathu n’kofunika ngako . Mau a Mulungu ali na mfundo zimene zimathandiza Akhiristu kusankha bwino mavalidwe . Ine ndi mkazi wanga sitinakhalepo ndi cimwemwe coposa ici . ” Ngati anazunza ine , inunso adzakuzunzani . ” ( Yoh . Yankho la funsoli ndi lofunika kwambili . N’nalimbikitsidwa cifukwa cokhalanso pamodzi na anthu a Yehova . ( Luka 2 : 51 ) N’zoonekelatu kuti iye anali kuganizila kwambili za mmene Mulungu adzakwanilitsila colinga cake cokhudza Mesiya . Mngeloyo anadutsa pa malo acitetezo , anatsegula zitseko , kenako anatulutsa atumwiwo ndi kutsekanso zitsekozo . Ena amakhulupilila kuti kumwamba kumakhala mizimu ya makolo akale amene afunika kulemekezedwa . ALI padziko lapansi , Yesu anapeleka citsanzo cabwino ca kudzimana . Kuopa dzina la Yehova kumatanthauza kum’lemekeza , kulemekeza zimene dzina lake limaimila , ndi miyezo yake . Zotulukapo zake zinali masoka okha - okha . Kulimbikitsa wolakwa kumam’thandiza kuti asamangodzimvela cisoni kapena kudziimba mlandu . 13 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi Adzathyola uta ndi kudula - dula mkondo . ’ Cioneka kuti zinali zosatheka kwa Mariya kuyenda na Yesu mu utumiki wake wa zaka zitatu na hafu . Mogwilizana ndi mfundo za m’Malemba zimenezi , tiyeni tiyelekezele kuti tikuona mmene moyo wa Inoki unathela . MAFUNSO ENA A M’BAIBULO AMENE AYANKHIDWA — Kodi Ngozi Zacilengedwe Ndi Cilango Cocokela kwa Mulungu ? Udindo wathu waukholo tinaulandila ndi manja aŵili ndipo tinali okonzeka kukhomeleza coonadi mwa ana athu okondeka . Katswili wina wa Baibulo analemba kuti : “ Ngati Kristu sanaukitsidwe , . . . ndiye kuti Akristu ndi anthu opusa kwambili amene amakhulupilila cinyengo cacikulu . ” Tyndale anakamba kuti ngati Mulungu angamulole kukhala ndi moyo kwa nthawi yaitali , iye adzaonetsetsa kuti ngakhale munthu wosaphunzila adziŵe Baibulo kuposa wansembe . Iwo anapulumuka pa nkhondo ya ku Dunkirk ndipo anali acisoni . Kodi Yehova akanacita ciani kuti athandize anthu popanda kunyalanyaza miyezo yake ? ( 1 Mbiri 16 : 27 ) Kuwonjezela apo , zinthu zabwino zimene atumiki ake amacita ‘ zimakondweletsa mtima wake . ’ — Miy . ( Ower . 11 : 35 - 39 ) Yefita ndi mwana wake anali okhulupilika , ndipo sanaganizilepo zophwanya lonjezo limene anacita kwa Mulungu Wam’mwambamwamba , ngakhale kuti anafunika kudzimana zambili kuti akwanilitse lonjezolo . — Ŵelengani Deuteronomo 23 : 21 , 23 ; Masalimo 15 : 4 . N’cifukwa ciani tiyenela kuyendela limodzi ndi gulu la Yehova ? ndi njila zatsopano ziti zimene atumiki a Mulungu akhala akugwilitsila nchito polalikila ? Ni mtendele wapadela uti umene tingakhale nawo ngati tiika maganizo pa zinthu zoyenela ? Ananionetsa mmene kuika zinthu za Ufumu patsogolo kumabweletsela madalitso na cimwemwe mu umoyo wa munthu . Mlembi wina wa Baibo anakambilatu za kuzilala kumeneku , kumene kuonekela bwino m’njila zambili . Ndiyeno , pa msonkhano wa cigawo wa mu 2009 , io anakhudzidwa kwambili ndi nkhani ina . ( Aroma 2 : 14 , 15 ) Buku lina lofotokoza Baibo limati liu la Cigiriki lomasulidwa kuti “ malangizo ” lingatanthauzenso “ kulela bwino mwana . ” Anauza milungu ya anthu a mitundu ina kuti ionetse umboni wakuti iyo ndi milungu yoona . Mwina Farao anali kufuna kumukopa na cuma cake , ndiyeno n’kukambilana ndi mlongosi wake kuti am’tenge kukhala mkazi wake . — Genesis 12 : 14 - 16 . Ndiyeno anali kuziyanika pa dzuŵa . Palibe cifukwa comveka cokwiila Yehova . Zimene Mose anakamba sizinali zopeleka ulemu kwa Yehova , Gwelo leni - leni la cozizwitsaco . Wofalitsa aliyense amafuna kulalikila mogwila mtima . Mu Nsanja ya Mlonda yacizungu ya June 1 muli funso yakuti : “ Kodi anthu amene akali ndi cizoloŵezi copepa fwaka ayenela kubatizika ? ” NYIMBO : 136 , 14 Zimapindulitsa onse ngati abale mumpingo adziŵa bwinobwino zimenezi , ndi kuyamikila atumiki a pa Beteli ndi nchito yao . — Ŵelengani 1 Atesalonika 2 : 9 . Yehova wapatsa Yesu mphamvu zoukitsa anthu amene ali ndi ciyembekezo cakumwamba . Ndipo adzaukitsanso mabiliyoni a anthu amene ali ndi ciyembekezo ca padziko lapansi . ( Aroma 6 : 7 ) M’mau ena , anthu akamwalila , sapitiliza kulangidwa cifukwa ca macimo ao . Kukonda abale na alongo athu n’kogwilizana ndi kukonda kwathu Yehova . Musacite kapena kuganizila zinthu zimene zingasokoneze ubwenzi wanu wamtengo wapatali ndi Yehova . M’masiku ano otsiliza , Yehova waphunzitsa anthu ake kukhala okondana kwambili . Iye anati : “ N’napeza cimwemwe cacikulu mu utumiki umenewu . Mwina munapola msanga , cakuti munaiŵala nthawi imene munadwala . Mwacionekele , Mulungu sindiye amacititsa zinthu zoipa zimene zimacitikila anthu , ndipo sindiye amacititsa kuti anthu azivutika . Kuyewa kunyumba . Mau a m’cigawo cimeneco amati mzinda wa Babulo udzakhala malo opanda anthu . Koma anali ndi cikhulupililo cakuti panthawi ina iliyonse , Yehova akhoza kuukitsa Isaki kuti malonjezo ake onse akwanilitsidwe . “ Ziwalo za thupi zimene zimaoneka ngati zofooka ndizo zofunika . ” — 1 AKOR . 17 : 10 ) Kodi tsopano mwaona cifukwa cake magazi ndi opatulika kwa Mulungu ? Komanso tili na mapulogilamu a pa zipangizo zamakono atatu cabe ovomelezeka . Mapulogilamu amenewa ni W Language , JW Laibulale , na JW Library Sign Language . Nanga kodi kukhala “ munthu wauzimu ” kumatanthauza ciani ? Kodi zocita zanga zimaonetsa kuti nimakhulupililadi kuti ano ni masiku otsiliza , ndi kuti mapeto a ulamulilo wa Satana ali pafupi ? Makonzedwe amenewa ndi ogwilizana ndi mfundo ya m’Malemba yonena kuti zoculuka zimene ena ali nazo zithandizile pa zimene ena akusowa , n’colinga cakuti “ pakhale kufanana . ” Tikatelo , Yehova adzatidalitsa . — Ŵelengani Genesis 39 : 21 - 23 . Tili ndi ufulu wodzisankhila zocita . N’ciani cingatithandize kukhala na mtima wofunitsitsa kudziŵika kwa Yehova ? Ndi mwai wotani umene tidzakhala nao pambuyo pa kuonongedwa kwa zipembedzo zonyenga ? Nanga anthu okhulupilika a Mulungu adzaonetsa bwanji kuti ndi osiyana ndi anthu ena ? Iye anati : “ Ineyo ndalankhula ndipo ndidzazicita . 146 : 3 , 4 ; Chiv . Woumba waluso amadziŵa bwino dothi limene akuseŵenzetsa poumba . Nayenso Yehova amatidziŵa bwino kwambili . Mwacitsanzo , kodi abale ndi alongo amene ali ndi cikhalidwe cosiyana ndi canu mumawaona bwanji ? N’ciani cinalepheletsa Kaini kupanga cosankha mwanzelu ? Ricky anasimba kuti : “ Pambuyo pa misonkhano , ndinafunsa Jacob mmene anali kumvelela ndi mpingo watsopano , popeza kuti munalibe acicepele a msinkhu wake . Mulungu woona yekha , amene dzina lake ni Yehova , ndiye angakambe zimenezi . Mwacitsanzo , pamene banja la Yakobo linali paulendo woosa wokakumana ndi Esau mbale wake amene anali kufuna kumupha pa nthawi ina , iye anatsimikiza kuti Rakele ndi Yosefe wacicepele aikidwa pamalo abwino kwa gulu lonse la a m’nyumba yake . Kodi kucita zambili potumikila Yehova mukali wacicepele , kungakuthandizeni bwanji kukonzekela maudindo ena am’tsogolo ? Onani zitsanzo za anthu amene anakhala olimba mtima pa mavuto mu Nsanja ya Olonda ya December 1 , 2000 , masamba 24 - 28 ; Galamukani ! Ngakale kuti Satana anasokoneza zinthu mu Edeni , Yehova anapeleka ciyembekezo kwa mtundu wa anthu mwa ulosi woyamba m’Baibulo . Kodi izi zigwilizana bwanji ndi mphatso ya dipo ? Koma Solomo anawononga ubwenzi wake wabwino na Yehova . ( Luka 10 : 17 , 21 ; Yohane 11 : 32 - 35 ) Mukamaŵelenga ndi kumvetsela nkhani za m’Baibulo zokhudzaYesu , muziikako nzelu kwambili ndi kuona m’maganizo mwanu monga ngati zinthuzo zikucitika inu mukuona . Koma kaŵili konse , Yesu anawadzudzula cifukwa ca khalidwe lawolo . ( Yohane 4 : 23 ) Mulungu akufuna kuti anthu otelo aphunzile coonadi ca Mau ake , Baibulo . — Ŵelengani 1 Timoteyo 2 : 3 - 5 . Kwa Mulungu , cikwati ni mgwilizano wa moyo wonse . Madzulo amenewo , iye ananipatsa malangizo abwino . M’bale wina wa ku England na mkazi wake , amene ni acikulile sakwanitsa kulalikila ku nyumba na nyumba cifukwa ca kufooka kwa thanzi . NKHANI YA PACIKUTO | MASOMPHENYA A ZINTHU ZA KUMWAMBA Motelo , ngati aliyense m’cikwati ‘ samangodzifunila zopindulitsa iye yekha basi , koma zopindulitsanso wina , ’ ndipo amapeleka mangawa a mucikwati osati mwa mwambo cabe koma mwacikondi , cikondico ndi cimene cingalimbitse cikwati cao . — 1 Akor . Kuuka kwa Kristu kumapeleka umboni wosatsutsika wakuti Yehova ndi wamphamvu , ndipo “ amapeleka mphoto kwa anthu omufunafuna ndi mtima wonse . ” ( Aheb . Abale a mu mpingo wina ku Honduras atayamba kusonkhana m’Nyumba ya Ufumu yatsopano , analemba kuti : “ Ndise okondwela maningi kukhala m’banja la Yehova la m’cilengedwe conse na kukhala m’gulu labwino la abale a pa dziko lonse . Onse amenewa atithandiza kuti tikhale na Nyumba ya Ufumu m’dela lathu . ” ( Mlaliki 5 : 10 ) Komanso , kusakhutila kungacititse munthu kunyalanyaza zinthu zofunika kwambili zimene zimacititsa munthu kukhala wacimwemwe , monga kukhala na nthawi yoceza na banja , mabwenzi , komanso kucita zinthu zauzimu . ( 2 Akor . 4 : 4 ) Ndipo tidzapitizabe kulalikila uthenga wabwino ngakhale kuti anthu alibe cidwi , amatinyoza , kapena kutitsutsa . — 1 Ates . Dzina la Mulungu lakuti “ Yehova , ” licokela ku mau aciheberi amene atanthauza “ Kukhala . ” 22 : 3 ) Conco , ngati mkulu wakukumbutsani malangizo opewela ngozi , muzilabadila . ( Agal . Muzikambilana nawo ofalitsa amene anacoka mu mpingo mwanu kukatumikila kosoŵa . Ku Dotana kunali kufupi ndi njila ya malonda yopita ku Iguputo , ndipo pasanapite nthawi gulu la apaulendo la Aisimayeli ndi Amidiyani linabwela . 19 : 5 , 6 . ( Gen . 45 : 9 , 10 ) Kwa zaka pafupifupi 100 , Aisiraeli anali kukhala mwamtendele ndi Aiguputo . Anali kukhala m’matauni aang’ono ndi kuŵeta nkhosa zao . Yesu anali wokoma mtima kwa akazi . Paradaiso ! Kodi ophunzila oyambilila a Yesu anali kusalidwa m’njila ziti ? Makolo muyenela kumakambilana ndi ana anu njila zimene angatetezele cikhulupililo cao ku sukulu . 7 : 26 ; 9 : 14 ) Komabe , kusamba kumene Aroni anali kucita kumaimila khalidwe loyela ndi lolungama la Yesu . 22 : 39 ; 1 Akor . 11 : 1 ) Tidziŵa madalitso ambili - mbili amene anthu angalandile ngati asankha kutumikila Yehova , ndipo timafuna kuti nawonso akalandile madalitso amenewo . Linafotokoza kuti kukhala wacifundo kumatanthauza “ kukhuzika mtima ndi kupeleka thandizo ” kwa ovutikawo . Ngakhale kuti tsopano ndikhala ndi mwamuna wanga , nthawi zina ndimafunikila kudziletsa kuti ndisacite zinthu zina . ” ( Aef . N’cifukwa ciani tikamba kuti zimene Yehova anacita poweluza Mose cinali cilungamo ? Mukatelo , cimakhala cosavuta kwa iwo kukhulupilila kuti ngati atsatila mfundo za m’Baibo nthawi zonse , zinthu zidzawayendela bwino . — Deut . N’cifukwa ciani pafunika kuti ena aphunzitsidwe ? 6 : 3 - 5 ) Komanso , anthu ena apanga maakaunti acinyengo pa intaneti na mawebusaiti abodza m’dzina la gulu lathu , la Bungwe Lolamulila , kapena mamembala ake . Patapita zaka zoposa 60 , Blossom anati : “ Kukamba zoona , sinidzaiŵala zimene zinacitika nthawi imeneyo ! ” Tikakumana ndi vuto , tifunika kuganizila zimene Yehova afuna kuti ticite . Kodi n’cifukwa cakuti munakumana ndi mavuto ena ake ? ( b ) Kodi mtendele umatithandiza bwanji kupitiliza kubala zipatso ? ( c ) Ndi malangizo ati amene akulu angagwilitsile nchito pophunzitsa ena ? Kodi kukonza bajeti kungathandize bwanji banja ? Tikutelo cifukwa lomba mau onse aŵili akuti “ odala ” m’vesiyi amamveka kuti akamba za anthu amodzi - modzi , “ anthu amene Mulungu wawo ndi Yehova . ” “ Kuyankha modekha kumabweza mkwiyo , koma mau opweteka amayambitsa mkwiyo . ” — Miy . 2 : 49 . Kuphunzila Baibo mwakhama ndi mosamala kungathandize Akhristu kukulitsa khalidwe la kudziletsa . Koma tsiku lina madzulo , Davide anaitanidwa . Kuyambila mu 1979 , Maureen watumikila monga mmishonale ku West Africa , kwa zaka zoposa 30 . ( Esitere 1 : 6 ) Nsalu zasilika zinali za mtengo wapatali , ndipo mwacionekele zinali kupezeka ndi anthu amalonda ocokela m’maiko ena a kum’maŵa kwa dziko lapansi . — Chivumbulutso 18 : 11 , 12 . Ndipo Natani ndiye mnzake amene Davide anafunikila panthawiyi . Abale ndi alongo athu ena amapilila masautso amene amabwela mwadzidzidzi . Funso limeneli n’lofunika kwambili . ( Afilipi 2 : 7 ) Yesu sanangokamba za Atate wake koma anationetsanso mmene Atatewo alili . ( Luka 10 : 38 - 42 ) Pamenepa , Yesu anali kuphunzitsa Marita mfundo yofunika ngako . Inde cimwemwe ndi cikhulupililo colimba ca Jairo ndi umboni woonekelatu wakuti kutumikila Yehova kumacititsa munthu kukhala wosangalala ngakhale ali pa mavuto otani . 2 : 19 , 20 ) Ndipo polembela mpingo wa ku Korinto , mtumwiyu anayamikila Tito kuti : “ Ndi mnzanga komanso ndikugwila naye nchito limodzi pothandiza inuyo . ” ( 2 Akor . Ponena za kapu ya vinyo , Yesu anauza ophunzila ake okhulupilika 11 kuti : “ Kapu iyi ikutanthauza pangano latsopano pamaziko a magazi anga , amene adzakhetsedwa cifukwa ca inu . ” Kuganizila kwambili mfundo za abale atatu amenewa kudzakuthandizani kumvela Mulungu ndi kukhalabe oyela . Limati : “ Mau alionse owola asatuluke pakamwa panu , koma alionse olimbikitsa monga mmene kungafunikile , kuti asangalatse owamva . ” — Aefeso 4 : 29 , 31 . Poyankha ndunayo inati : “ Ndingamvetse bwanji popanda wondimasulila ? ” Ndipo Baibo imatiphunzitsa mmene tingapangile zosankha mwanzelu . 8 : 27 14 - 16 . ( a ) Kodi Aisiraeli anakhala motani mtundu wa mboni za Yehova ? ( Chiv . 18 : 4 ) A “ nkhosa zina ” akuthandiza Akristu odzozedwa kupempha anthu otalikilana ndi Mulungu kuti ‘ agwilizanenso ’ ndi iye . — Yoh . Pamene anali padziko lapansi , Yesu anaonetsa kuti ndi wodzicepetsadi mwa mau ake ndi zocita zake . Baibulo la Dziko Latsopano lidzakhalanso m’zinenelo zambili mtsogolomu . 4 , 5 . ( a ) N’cifukwa ciani tikamba kuti kudzipeleka ni udindo wa Mkhristu aliyense payekha ? Mu 2010 , Richard wa zaka 65 , anacoka ku United States ndi kupita ku Guam . Baibulo limaonetsa kuti Ufumu wa Mulungu unayamba kulamulila kumwamba mu 1914 . Khadi la cipani Koma kodi kusamalila okalamba ndi udindo wa ndani ? Patsiku lapadela limenelo , ciŵelengelo ca ophunzilawo “ cinaonjezeka ndi anthu pafupifupi 3,000 . ” Ana anu acinyamata adzaona kuti simunapange lamulo kapena cosankha cabe cifukwa cakuti muli ndi mphamvu yocita zimenezo , koma cifukwa cakuti muli ndi zifukwa zomveka . Pofuna kulepheletsa cifunilo ca Mulungu , Satana Mdyelekezi anasonkhezela anthu kuti apanduke . Kucita izi kungamuthandize kuti akhalenso wolimba mwauzimu . ( Sal . Mofanana ndi Yosiya , acicepele ayenela kuyamba kuphunzila za Yehova akali aang’ono . Mumadziŵa bwanji kuti Yehova amayankha mapemphelo ? Dokota wina anati kuseŵenzetsa malangizo a m’Baibo kuli monga kuseŵenzetsa buku la m’ma 1920 pophunzitsa ana a sukulu za sayansi . Kuti mudziŵe zambili zokhudza zimene Baibo imakamba pa nkhani ya moyo na imfa , onani nkhani 6 m’buku yakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni yofalitsiwa na Mboni za Yehova . Komabe , sanapite patsogolo , ndipo sanali kupita kumisonkhano . Kuyambila pa Pentekosite wa mu 33 C.E . , Akristu anali kukumana nthawi zonse kuti alambile Yehova . Kupilila Cisoni 5 Banja lingasankhe mmene lingapelekele cisamalilo , cifukwa banja lililonse lili ndi mavuto ake . ( b ) Nanga mwatsimikiza mtima kucita ciani pamene muli mu ulaliki ? Anthu amene adziŵa Yehova na kuyamba kum’tumikila sacita zinthu ngati anthu a m’dzikoli , amene amaoneka ngati odzipeleka kwa Mulungu , koma amakana kuti mphamvu ya kudzipelekako iwasinthe . 3 : 15 ) Pamene Yesu Khiristu , amene ni “ mbeu ” yolonjezedwa , anatsegula njila yamoyo wakumwamba , anthu okhulupilika amenewa anali atafa kale . N’cifukwa cake mutu na mau ena m’nyimboyi zinasinthiwa . Sindidzaiwala zimene zinacitika tsiku lina mu 1971 . Ngati zimenezi zakucitikilani , pemphani Mulungu kuti akuthandizeni kukhala olimba mtima ndi kuuza ena momveka bwino cifukwa cake simutenga mbali m’ndale . Tinaphunzilanso zambili za cilengedwe , ndipo zimenezi zinandithandiza kuyamikila nchito ya Mlengi wathu . A Inoki : Coyamba ndifunseko , kodi munakulila m’banja lacikristu ? Iye sanayende naye kwa zaka 70 kapena 80 cabe , koma anayenda naye kwa zaka pafupi - fupi 600 ! Pamene Yesu anakamba kuti , “ Musaganize kuti ndinabweletsa mtendele , ” anatanthauza kuti omvela ake anafunika kuganizila mavuto amene angakumane nawo cifukwa comutsatila . Paulo analembela Akristu a ku Roma kuti : “ Cimene tiyenela kupemphelela monga mmene tiyenela kupemphela sitikucidziŵa , koma mzimu umacondelela m’malo mwathu ndi madandaulo amene sitinathe kuwafotokoza . Ndipo cinthu cimene cinali cofunika kwambili kwa iye , ndi kukhala ndi mwai wothandiza poyeletsa dzina la Mulungu ndi kuonetsa kuti Iye ndiye woyenela kulamulila . 10 : 16 ) Kutalitali ! Mu ulosi umenewu , zinthu zoipa zimene zikucitika zikuimilidwa ndi okwela pa akavalo atatu amene akuyendetsa akavalo ao mofulumila kwambili ndipo akutsatila Yesu Kristu m’mbuyo . — Chiv . ( Deuteronomo 5 : 6 - 10 ) Masiku ano , pali mitundu yambili ya kulambila mafano , ndipo ina sitingaidziŵe mwamsanga . Mmene anthu amatiganizila zimadalila zimene ‘ aona ndi maso ’ awo . ( 1 Sam . ( Genesis 2 : 16 , 17 ) Mau awa amaonetsa bwino kuti Adamu akanamvela lamulo la Mulungu , sembe sanafe . Akanapitiliza kukhala m’munda wa Edeni . Atumiki a Mulungu amawakhulupilila kwambili mau amenewa , ndipo amazimva otetezeka kudziŵa zimenezi . Mogwilizana ndi vesili , kodi ndi njila imodzi iti imene tingayandikilile Atate ? Iye anali kuyamikila khama lawo . Ndipo zimenezi zinamuthandiza kwambili cakuti anayamba kuwakonda . M’modzi wa opezeka pa msonkhano dzina lake Beulah Covey anati : “ Anchito odzifunila amene amagwila nchito modzipeleka amathandiza kuti zinthu ziyende bwino . ” Yesu anamusankha kuti akhale mtumwi . Komabe , sindidzaleka kuwapemphelela kuti aphunzile coonadi . Nkhaniyo itayamba , palibe amene anadziŵa kuti m’mwamba kutsogolo kwa pulatifomu kunali cinsalu copindidwa bwino . Yesu anali kumvetsa mavuto a ena , ngakhale amene iye sanakumanepo nao . 7 , 8 . ( a ) N’cifukwa ciani Ayuda ambili m’zaka za m’ma 200 B.C.E sanali kumvetsetsa Malemba Aciheberi ? Mkwati , Yesu Kristu , wavala zovala za cikwati zaulemelelo ndiponso zacifumu . 3 : 17 ) Conco , ngati Mkristu ali ndi udindo wosamalila osoŵa , naonso mpingo uli ndi udindo umenewu . Koma si zokhazo . “ M’masiku ovuta amenewo , n’nali kupempha Yehova kuti anithandize kupilila ndi kukhala na mtendele wa m’maganizo . Ndinakonza kasitandi kogulisilapo zipatso pa nyumba pathu , ndipo pamalopo ndinali kupasunga paukhondo . 6 : 1 , 2 ) Pocita phunzilo laumwini , muyenela kucita khama kuti mupeze mfundo zatsopano ndi zothandiza . Ngati n’conco , musataye mtima . N’cifukwa ciani kumasulila Baibulo m’zinenelo zina n’kofunika kwambili ? Pa utumiki wake , Yesu anakamba za Ufumu nthawi zoposa 100 . Cinthu coyamba cimene Mfumu ya Mulungu yatsopano inacita , cinali kucita nkhondo ndi Satana , Mdani wamkulu wa Atate wake . Conco , ifenso tiyeni tizilimbikitsa akulu , kuphatikizapo amadela , cifukwa cogwila nchito molimbika kuti asamalile nkhosa za Mulungu . Mukauza mkristu mnzanu kuti akapemphe thandizo kwa akulu , ndiye kuti mukucita zinthu mokoma mtima ndiponso ndinu wokhulupilika kwa Yehova TIKUKHALA m’nthawi yosautsa kwambili . ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Malinga ndi mmene inuyo mwaonela , n’ciani cionetsa kuti anthu ali ndi mtima wankhanza ngati Satana ? ( Mat . 23 : 23 ) Mosiyana na Afarisi , amene anali odzilungamitsa , Yesu anali kudziŵa bwino colinga ca Cilamulo , komanso makhalidwe a Mulungu amene anali kuonekela pa lamulo lililonse la m’cilamuloco . Mofanana ndi mautumiki ena opatulika , kutumikila pamodzi ndi abale pa nchito yomanga kumabweletsa cimwemwe . N’cifukwa ciani mapiliwo ni amkuwa ? ( 1 Yohane 3 : 8 ) Dongosolo la zinthu lamakono limene ndi ladyela , cidani ndi macitidwe ena oipa lidzaonongedwa . Pambuyo pake , io anayamba kukambilana maulosi ndi mmene anakwanilitsidwila . Aphunzitsi okoma mtima amaona ophunzila monga “ anchito anzao ” ndiponso mphatso zamtengo wapatali mumpingo osati monga anthu opikisana nao . ( 2 Akor . 1 : 24 ; Aheb . NYIMBO : 75 , 74 Nili kumeneko , n’naganiza kuti : ‘ Kaya n’dzacila kaya ? Ngati kutsatila Yesu kwabweletsa “ lupanga ” m’banja lanu , dalilani Yehova kuti akuthandizeni kupilila . ( Yes . Coyamba , tiyeni tikambilane za Asa , ndi kuona mmene Mau a Mulungu angatithandizile pa umoyo wathu . Nchito yophunzitsa anthu nimaikonda cifukwa nimaona mmene mzimu woyela umathandizila anthu kusintha umoyo wawo . ” — 1 Ates . Kodi Yehova amadalitsa bwanji anthu amene amalimbitsa cikhulupililo cao ? Komabe , ganizilani anamwino kapena kuti azamba aciheberi Sifira ndi Puwa , amene mwina anali kutsogolela pa nchito ya unamwino . Nthawi zina , muzimupempha kuti azikhala nanu pa kulambila kwa pabanja pamodzi ndi banja lake . Iye samangokhalila kutiongolela tikalakwitsa , koma amatiphunzitsa . Lemba la Chivumbulutso 19 : 11 limati : “ Nditayang’ana ndinaona kumwamba kutatseguka , kenako ndinaona hatchi yoyela . ( Aroma 5 : 12 ) Timafa cifukwa tinatengela ucimo kwa makolo athu oyambilila , osati cifukwa cakuti Mulungu anakonzelatu ‘ mapulani ’ ena osamvetsetseka . Ndiyeno M’bale Rutherford anafuula kuti : “ Ndiye pitani mukalalikile , inu ana a Mulungu wam’mwamba - mwamba ! Iwo amakhulupilila kuti mofanana ndi tate wa mu fanizo la mwana woloŵelela , Yehova amayembekezela mwacidwi kulandila anthu olapa . Yesu sanalole cinthu ciliconse kum’sokoneza kulalikila . Ngakhale malangizo a tsopanowo ni njila ina imene Yehova adzaonetsela kukoma mtima kwake kwakukulu . 1 : 8 ) Buku lina lofotokoza Baibulo linati : “ Kuonetsa cifundo kumafuna zambili kuposa kungomvela cisoni anthu osoŵa . ” ( Mac . 26 : 23 ) Komabe , pali ena amene analonjezedwa kuti adzaukitsidwa kuti akakhale kumwamba monga zolengedwa zauzimu . Pulogilamu imeneyi , imene idzatenga ola limodzi , idzaphatikizapo nkhani ya m’Baibo imene idzafotokoza cifukwa cake imfa ya Yesu ni yofunika . Bwanji ngati makolo anthu okalamba adzafunikila cisamalilo cathu ? Iye anadzifunsa kuti , ‘ Nidzapitiliza bwanji kucita utumiki wa upainiya , umene nimaukonda kwambili ? ’ ( Miy . 28 : 26 ) Zitsanzo za m’Baibo zimaonetsa kuti ngati munthu amangotsatila mtima wake pocita zinthu , amakumana ndi mavuto . Pamene ndinali mwana ndinali kusamalidwa ndi ambuye anga cifukwa cakuti makolo anga anali kuseŵenza masana ndi usiku kuti apeze ndalama zakuti adzagulile nyumba yabwino . Ngati mwaona cinacake pa Intaneti cimene cakudetsani nkhawa , pemphani Yehova kuti akupatseni nzelu . Ngakhale kuti Nowa , Danieli , na Yobu anakhalako m’nthawi zosiyana , ndipo anakumana na mavuto osiyana - siyana , onse anapilila . ( Luka 10 : 21 ) Baibo inalembedwa m’njila yakuti anthu okhawo amene ali na maganizo oyenela azitha kumvetsetsa uthenga wake . Janet anati : “ Usiku m’pamene ndimakhala ndi nkhawa kwambili . Ca pa nthawi imeneyi , m’bale Nikolai Chimpoesh , amene anacokela ku Moldova , anaikidwa kukhala woyang’anila dela . Iye anatumikila pa udindowu kwa zaka pafupi - fupi 30 . Onani zitsanzo zina izi za cikondi caciphamaso . Tonse tingavomeleze kuti panthawi ina , munthu aliyense anaonetsapo ena mwa makhalidwe amenewa . Mwamuna wanga atabwelako , ndinafunika kukhala wogonjela . Posacedwa , zolengedwa zauzimu za nkhanza zimenezo zidzacotsedwapo . Dzina la m’Baibo pa Mtsuko Wakale , Mar . Kodi n’ciani cinawalimbitsa mtima ? Sadirake , Mesake ndi Abedinego , anyamata atatu amene anali oopa Yehova , anakana kutsatila lamulo limenelo . Ndi nchito yotani imene Yehova anapatsa Yesaya ? Nanga Yesaya anailandila bwanji ? “ Yehova adzacilikiza wonyozekayo pamene akudwala pabedi lake . ” — SALIMO 41 : 3 . ( Ŵelengani Levitiko 8 : 22 - 24 . ) Izi zikutipatsa cithunzi ca nthawi imene ciukililo copita kumwamba cidzacitika . Iye anaonetsetsa kuti anthu amene anapita kukapeleka ndalamazo ‘ akusamalila zinthu zonse moona mtima , osati pamaso pa Yehova pokha ayi , komanso pamaso pa anthu . ’ Kodi tiphunzilapo ciani pa cocitikaci ? Mwai wathu wochedwa ndi dzina la Mulungu umafuna kuti tizicita zinthu zoonjezeleka ziti ? Kodi cinam’thandiza n’ciani kuti ayambe kukhulupilila kuti Mulungu amam’kondadi ? Yehova amatikonda kwambili ise anthu ndipo amationa kuti ndise ofunika ngako . PACIKUTO : Anthu ambili amapita ku Copán kukaona mabwinja ocititsa cidwi , koma Mboni za Yehova kumeneko zimathandiza anthu kuyembekezela zinthu zabwino mtsogolo Tsiku lina usiku , ndili ku misonkhano ya Mboni , gulu la anzanga linapita ku kumalo ovinila . N’cifukwa ciani Akristu ena a ku Korinto anali kudya zizindikilo za pa Cikumbutso mosayenelela ? Koma nkhanza zimenezo zinangolimbitsa cosankha canga ‘ comvela Mulungu monga wolamulila , osati anthu . ’ — Mac . Anthu olimbika sapewa kugwila nchito . Cikalata ca ku Iguputo ca mu 1200 B.C.E . , cinakamba kuti m’dziko la Kanani munali asilikali ena oopsa amene anali aatali mamita 2.4 . mumakhalako nkhani zofunsa asayansi ndi akatswili ena kuti afotokoze cimene cinapangitsa kuti ayambe kukhulupilila Mulungu . Izi zinacititsa kuti asinthe modabwitsa . Iye anakamba kuti : “ Pakuti iwo ndi mtundu wopanda nzelu , ndipo ndi osazindikila . 17 , 18 . ( a ) N’ciani cingakuthandizeni kutenga coonadi kukhala canu - canu ? Kodi Baibulo ndi lofala bwanji masiku ano ? 16 : 25 - 33 ) Pa ulendo wake waciŵili waumishonale , ca mu 50 C.E . , Paulo anafikanso ku mzinda wa Filipi . M’kupita kwa nthawi , tinayamba kulembelana makalata . Ziyeneletso zina za nchito yabwino zipezeka pa lemba la 1 Timoteyo 3 : 2 - 7 ndi Tito 1 : 5 - 9 . Sisera anafika kuhema wa Hiberi ali wotopa kwambili . Conco ananditenga ndi kupita nane ku polisi ndipo anayamba kundimenya . Ndipo anthu 600 sauzande amene sakoka fodya amafa caka ciliconse cifukwa copuma utsi wake . Conco , munthu wodzicepetsa amakhala ndi maganizo oyenela ndipo amayesetsa kucita zimene angathe . N’cifukwa ciani cingakhale covuta kupewa kutenga mbali m’ndale ngati timakonda kwambili zinthu zakuthupi ? Dzina limeneli limatanthauza kuti “ Yehova ndi Mtendele . ” Koma koposa zonse , tadziŵa Yehova Mulungu amene amatikonda monga atate wathu . — Yakobo 4 : 8 . Conco , n’naleka kucitila saliyuti mbendela ndi kuimba nyimbo ya fuko . Wophunzila asanabatizike , afunika kukhala na cikhulupililo . Ndaona mmene cikhulupililo ca Jairo camucititsila kukhala ndi moyo waphindu ngakhale kuti ali ndi umoyo wovuta kwambili . ” Anthu amene mufuna kuti akhale mabwenzi anu ayenela kukhala ndi cikhulupililo colimba ndiponso omvela Yesu . Mu ulosi wa Ezekieli , Yesu anachulidwa kuti “ Mtumiki wanga Davide . ” ( Ezek . Baibo imene poyamba inali yosavuta kumva , m’kupita kwa zaka imakhala yovuta kumva . Zinthu zina zokongoletsela pa cihema zinali zopangidwa mwaluso . Pamsonkhano umene unacitika ku Sin - le - Noble mu 1926 , anthu 1,000 anapezeka pa mapulogilamu a Cipolishi , ndipo 300 anapezeka pa ya Cifulenci . Mwacitsanzo , cifukwa cokonda Mulungu , tiyenela kuuzako ena za iye ndi kuyankhapo pamisonkhano . ( Luka 11 : 1 - 4 ) Pamenepa Yesu anatithandiza kudziŵa zinthu zimene tifunika kupempha . Pezani njila yothandizila mkazi wanu nchito za pakhomo . Chaputa 11 ca buku ya Aheberi cimachula maina 16 a amuna ndi akazi amene anali na cikhulupililo . Nkhani ziŵilizi ziyankha mafunso ofunika amenewa . Abigayeli Hana nayenso anasunga mokhulupilika lonjezo limene anapanga kwa Yehova . Popeza kuti mfundo za Yehova n’zolungama nthawi zonse , n’zosatheka iye kuweluza mopanda cilungamo . * Kuti tipeze yankho , coyamba tiyeni tione mmene Yesu anaphunzitsila ophunzila ake kupemphela . Mu 1957 , n’nalandila ciitano cakuti nikapezeke pa msonkhano wa Mboni za Yehova . Msonkhanowo unali kucitikila m’bwalo la maseŵela limene n’nali kuchailamo baseball . Mwacitsanzo , tingagonjetse bwanji maganizo olefula ? Poyankha , kodi Yehova anawauza ciani ? Ucengeteni mwayi umenewo , ndipo pitilizani kuyenda ndi Yehova modzicepetsa kwamuyaya . Iye ayenela kuti anadabwa kwambili m’mawa mmenemo kuona atate ake amene anali wokalamba koma amphamvu akuyenda cotsimphina . ( Akol . 3 : 13 ) Kukamba zoona , timafunika kuyesetsa kukhala ofatsa ndi oleza mtima kuti tikwanitse kumvela lamulo limeneli . Mboni za Yehova nazonso zimachula dzina la Yesu . Kadontho kamodzi ka madzi kamacita zocepa , koma madontho ambili amanyowetsa nthaka . Baibulo . Ngakhale kuti malamulo a Mulungu anali acindunji , malamulowo aonetsa kuti iye ndi wacikondi ndi wololela . Kodi umoyo ukanakhala bwanji Mulungu akanapanda kutikonda ? Yehova ndiye yekha amene ali woyenela kulamulila cilengedwe conse . Mwacitsanzo , pogwila mau m’mipukutu , Paulo anali kukamba kuti , “ monga mmene Malemba amanenela kuti ” kapena , “ monga Yesaya ananenelatu kuti . ” Ngati mufuna kudziŵa zambili , mungalembe kalata ku ofesi ya nthambi ya Mboni zaYehova ya m’dziko lanu . Anamuuza kuti atenge ndodo yake na kukamenya thanthwe ku Horebe , kuti madzi akatuluke m’thanthwelo . 2 : 11 ) Mneneli Zefaniya anati : “ Tsiku lalikulu la Yehova lili pafupi . N’nayamba kuganiza kuti mwina Sauli ndi Davide anaimilila pa malo amene ine n’naima . Ŵelengani Luka 16 : 10 - 13 . “ Kukamba zoona , sindinali kudziŵa kuti io ndani ndipo sindinali kudziŵanso zimene amakhulupilila . ” — Cecilie wa ku Esbjerg , Denmark . ( Dan . 3 : 16 - 18 ) Anthu a msinkhu uliwonse angaope akaopsezedwa , koma acicepele ndi amene amaopa kwambili kucita zinthu mosiyana ndi anzao . Komanso , Malemba Aciheberi na Malemba Acigiriki Acikhristu , onse amalangiza ana kuti azilemekeza makolo awo . — Eks . Yesu anaphunzitsa kuti maziko okha a m’Malemba othetsela cikwati ndi pamene wina wacita cigololo , ndipo mnzake wosalakwa wasankha kuti asam’khululukile . ( Mat . 19 : 9 ; Aheb . 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani n’kofunika kuti Akhristu azikhala okhulupilika kwa Mulungu ? Ngati timagonjela ndi kumvela ndi mtima wonse malangizo amene akulu amatipatsa , Mulungu adzatidalitsa . — Aheb . Kodi fanizo la Yesu la khoka limatanthauza ciani ? ( Afilipi 1 : 10 ) Kodi zinthu zofunika kwambili ndi ziti ? Izi zimatidziŵikitsa kuti ndise Akhristu oona , ndipo n’zogwilizana ndi malangizo amene mtumwi Paulo anauzilidwa kulemba akuti : “ Musabwezele coipa pa coipa . . . . Kuonjezela pamenepo , tingayambe kukonda munthu amene si mwamuna kapena mkazi wathu cifukwa cakuti ndife opanda ungwilo ndipo mtima wathu ndi wonyenga . Ngati mumamvela conco , ganizilani za munthu wokhulupilika Yobu . Pali pano , tikali kucilikiza mpingo wa m’dela la Bronx . N’zosangalatsa kwambili kudziŵa kuti Yehova akusamalila zosoŵa zakuuzimu za anthu ake onse , ngakhale amene ali pazilumba zimene zili pakati pa Nyanja ya Pacific . Yesu Khiristu anali kumwamba akalibe kubwela padziko lapansi . Mulungu anauza Abulahamu ndi Sara kuti asamuke mumzinda wa Uri ndi kukakhala ku dziko lacilendo . Yakobo anauzilidwa kulemba kuti : “ Mulole kuti kupilila kumalize kugwila nchito yake , kuti mukhale okwanila ndi opanda cilema m’mbali zonse , osapelewela kalikonse . ” Atumiki a Yehova ndife osangalala kwambili cifukwa caka ciliconse anthu oposa 250,000 amabatizidwa . Kevin , tate wa ana aŵili , wina wa zaka 5 ndi wa zaka 8 , anapeza njila zina zothandizila ana ake kuti azipindula ngakhale kuti sanali kumvetsetsa pamisonkhano . Akatswili ena amalimbikitsa makolo kuti nthawi zonse aziyamikila ana awo . 91 : 2 . Kwa anthu amene amadziŵika ndi Mulungu , mfundo za Yehova zinganenedwe mwacidule m’mbali ziŵili izi : ( 1 ) Yehova amakonda anthu okhulupilika kwa iye , ndipo ( 2 ) Yehova amadana ndi cisalungamo . Kodi ndine wodziletsa ? Anthu a Mulungu akupitilizabe kuculuka ngakhale kuti ali ndi mdani wamphamvu , Satana . Rute anagwada pamaso pa Boazi na kum’funsa cifukwa cake anamuonetsa cisomo cotelo , iye pokhala mlendo . Mwacitsanzo , ganizilani mmene zosoŵa zathu za kuuzimu zimaonekela m’mapempho atatu omalizila m’pemphelo la citsanzo . kuti amukope cidwi pa Mau a Mulungu 21 : 1 - 6 ) Conco panthawiyo , Davide anali ‘ kupemphapempha cakudya . ’ Tingaonetse bwanji kuti ndise ofatsa ndi oleza mtima ? Ndinakhudzidwa kwambili kuti Yehova anatipatsa thandizo pogwilitsila nchito munthu wotsutsa amene mwacionekele anali kuŵelenga zofalitsa zathu . Iye anali wofunitsitsa kukhalabe ndi mphunzitsi wake mulimonse mmene zikanakhalila . “ Mtanda wonsewo ” wa ufa umaimila mitundu yonse , ndipo kufufuma kumaimila kufalikila kwa uthenga wa Ufumu kudzela m’nchito yolalikila . Koma anthu ena amaona kuti maganizo amenewo ni olakwika . Nkhani zimene zingathandize Akristu okhulupilika kupilila pamene wacibale wao wacotsedwa zinafalitsidwa mu Nsanja ya Olonda ya September 1 , 2006 ( tsamba 17 mpaka 21 ) , ndi ya January 15 , 2007 ( tsamba 17 mpaka 20 ) . Timathela nthawi yambili kuthandiza ena kuti adziŵe Baibo . ofalitsidwa m’zinenelo 100 , amatithandiza kudziŵa zambili zokhudza cilengedwe ca Yehova . Amationetsanso mmene tingatsatilile uphungu wothandiza wa m’Baibulo . ( Miy . Mwina mukudziŵa kuti Baibulo ndi buku la mbili yakale . Kumeneko , Sisera anagona cifukwa anali atatopa kwambili kunkhondo . Conco , mmalo mokhumudwa cifukwa colephela kucita zinthu zina , sangalalani ndi zimene mumakwanitsa kucita . Conco , tiyeni tizikamba mau olimbikitsa kwa ena . Tikatelo , Yehova adzasangalala . Koma anali kulambila Mulungu wao , Yehova . — Genesis 24 : 50 . Popeza kuti uthenga wa m’Baibo ni wofunika kwambili , si bwino kudalila cabe nzelu zathu kuti timvetsetse zimene timaŵelenga m’Baibo . Kodi ziwanda zaonetsa bwanji kuti ndi zamphamvu ? Mipingo yambili imasonkhana m’malo olambilila okongola ndi ocititsa cidwi kwambili ochedwa Nyumba za Ufumu . Ulosiwu unayamba kukwanilitsika mu 1919 pamene Mulungu anayamba kugwilizanitsa anthu ake pang’ono - pang’ono . Zimenezi sizingacitike . Komanso , ena amavutika ngakhale kupezela mabanja awo zinthu zofunika kwambili pa umoyo . Pa nkhani zaconco , kodi tingadziŵe bwanji zimene zili zovomelezeka na zokondweletsa kwa Mulungu ? ANTHU TINALENGEWA MWAPADELA MANINGI , TIMAKWANITSA KULEMBA , KUPENTA , KUPANGA ZINTHU , NA KUGANIZILA MAFUNSO OFUNIKA KWAMBILI MU UMOYO MONGA AKUTI : N’cifukwa ciani zinthu zinalengewa ? Conco , Sebina anali na udindo waukulu . ( Yes . Colinga cimene mnyamatayo anayambila kuphunzila Baibulo cinali cakuti akhale pacibwenzi ndi Ratana . Umu ni mmene zinthu zakhalila kungoyambila pamene anthu analengedwa pa dziko lapansi . Iwo amatamanda kwambili atsogoleli acipembedzo , andale , akatswili a zamaseŵela , ndi ena , ndipo amafika powaona monga ni milungu . Nanga n’ciani cidzacitika kwa odzozedwa amene adzalephela kukhala maso ndi kukhala okhulupilika cisautso cacikulu cisanayambe ? Conco , Yesu anabwezeletsa zinthu zimene Adamu anataya . Ngakhale n’conco , Esitere anakhalabe waulemu ndi wodzicepetsa . N’cifukwa ciani zinthu masiku ano zasintha kwambili ? Kupempha thandizo n’kofunika kwambili ngati tikulimbana ndi zilakolako zoipa cifukwa copenyelela zamalisece . ( b ) N’ciani cimene cingatithandize kuti tikhalebe pa mtendele na Mkhristu mnzathu amene watilakwila ? Conco , ophunzilawo anaphunzilapo kuti naonso anayenela kukhala odzicepetsa ndi kudalila Yehova . Ndipo wokhala pampando wacifumu anati : ‘ Taonani ! Kuti tipeze yankho , tiyenela kudziŵa mmene Aroma anali kuonela zacipembedzo . Ndani ena amene anapeleka citsanzo cabwino pa nkhani yopilila ? 40 : 31 ; 1 Ates . Popeza ndife mbadwa za Adamu , tinatengela ucimo ndipo matupi athu ndi opanda ungwilo , conco timafa . 15 : 30 - 34 ) Tengelani citsanzo ca Davide . M’malo molola nkhawa kukufooketsani , citani zimene mungathe kuti mulimbane ndi vutolo . Ndiyeno , siyani zonse m’manja mwa Yehova . Baibulo limakamba za ngozi imene ikubwela . Limati : “ Kudzakhala cisautso cacikulu cimene sicinacitikepo kucokela pa ciyambi ca dziko mpaka tsopano , ndipo sicidzacitikanso . ” Kukambilana moona mtima ngati wodwalayo angafunike kumuika ku mashini opumila , kumucita adimiti m’cipatala , kapena kulandila mankhwala akuti - akuti , kungacepetse mikangano komanso kudziimba mlandu kumbali ya acibanja amene akupangila zosankha wodwala amene sakwanitsa kucita ciliconse . Kukhala wacimwemwe sikutanthauza kukhala wansangala cabe kapena woseka - seka . 16 Lolani Malamulo a Mulungu na Mfundo Zake Kuphunzitsa Cikumbumtima Canu Ndife okondwa kuti Yesu anati : “ Mudzadziŵa coonadi , ndipo coonadi cidzakumasulani . ” Mwacitsanzo , ngati sitinamvetsetse mau olembedwa pa botolo la mankhwala , tingakumane na mavuto aakulu . Fotokozani zimene zinacitika kuti mngelo wina akhale Satana . Koma m’madela ena , alendo komanso eni ake nyumba , onse amadya zakudya zolingana . M’zikhalidwe zinanso , alendo amatengako mphatso popita kukaceza . Pa misonkhano ya mpingo imeneyo komanso yadela ndi yacigawo , timaphunzila mfundo za m’Baibulo zimene zimalimbitsa cikhulupililo cathu mwa Mulungu ndi malonjezo ake . — Aheb . Koma ngakhale zinali conco , Mulungu sanatikane ndipo sanasinthe colinga cake pa anthu ndi dziko lapansi . Mwacitsanzo , mbusayo anali kukonda mmene mtsikanayo anali kukambila ndi anthu ena . Aliyense amakumana ndi mavuto osiyanasiyana amene mwina ife sitinakumanepo nao . Komanso , mungadzipeleke kugwila nchito zina za pampingo , monga kuyeletsa ndi kukonza zowonongeka pa Nyumba ya Ufumu . Koma a nkhosa zina ali na ciyembekezo cosiyanako . Timadziŵanso kuti sindife aulesi . Iye anaona kuti Mulungu ndiye anacititsa mavuto ake , ndipo sanaganizilepo kuti Mulungu angakhale na njila ina yothetsela mavutowo . Nkhani yake ndi yakuti : N’cifukwa ciani nchito yolalikila za Ufumu ndi yofunika kwambili ? Iwo anakwanitsa kuleka makhalidwe oipawa cifukwa analola mphamvu ya Mau a Mulungu ndi mzimu wake woyela kutsogolela maganizo ndi mitima yawo . 17 : 12 - 14 ; 19 : 11 , 14 , 15 ) Koma Mphukila asanapeleke ciweluzo , ali na nchito yaikulu yofunika kugwila . Cisautso cacikulu cimene sicinacitikepo m’mbili yonse ya anthu cifika posacedwapa . Mwacitsanzo , buku lina limakamba kuti “ asayansi apita patsogolo kwambili m’kafuku - fuku wawo ” pa nkhani imeneyi . Muzithandiza odwala na okalamba . Ataona kuti Aisiraeli ena am’pandukila , Rehobowamu anasonkhanitsa asilikali ake kuti akawathile nkhondo . Kuti ana amvetsetse coonadi , pali zambili zimene zimafunikila . Kupezeka pa misonkhano wiki iliyonse pakokha si kokwanila , olo misonkhanoyo itakhala kuti imacitika m’citundu codziŵika . Mwacitsanzo , ng’anga ina yochuka ku Madagascar , inaona kuti Mboni za Yehova ndi zamtendele . Ndiye cifukwa cake tiyenela “ kukhala maso ndi kucenjela ndi kusilila kwa nsanje kwamtundu uliwonse . ” Iye anali kudziŵa zinthu zimene anthu amafunikila tsiku ndi tsiku . 1 : 11 ; 1 Yoh . 4 : 8 ) Kuti tikhale osangalala , tiyenela kuonetsa cikondi ceniceni kwa anzathu , kuganizila zotulukapo za zocita zathu , ndi kupewa nkhawa . [ Mau apansi ] Mau akuti “ mana ” acokela ku mau aciheberi akuti “ man hu ’ ? ” A Joseph ndi ana ao anakanilatu kusintha maganizo ao pankhani yokhudza kulambila . Poceleza alendo ndi popatsa ena mphatso , kodi colinga canga cimakhala cabwino ? — Mat . Ndi mfundo yotani imene Yesu anaphunzitsa ophunzila ake ? Pambuyo pochula kuti Paulo anali kugwila nchito yopanga matenti , Baibo imafotokoza kuti iye anaika patsogolo maka - maka nchito yolalikila ndi kuphunzitsa anthu . NGATI ndinu kholo , mwadziŵa mmene zimamvekela mwana akakuuza zimene tachula m’mau oyambililawa . Koma kodi n’ndani adzatsogolela gulu lankhondo lakumwamba la Yehova ? Mu 1926 , Arthur Guest anamanga banja ndi Hazel Wilkinson , amene amayi awo anaphunzila coonadi mu 1908 . Ndipo pulojekita ya seŵelo la “ Eureka Y ” sinali kugwilitsila nchito malaiti , koma toci . Koma seŵelo la “ Eureka Y ” linali ndi nkhani zonse zojambula ndi zithunzi zokongola . ( Yesaya 11 : 6 - 8 ; Akolose 3 : 9 , 10 ) Tsopano tili m’Paradaiso wauzimu . Yohane anati : “ Iwo anapita kukalalikila za dzina la Mulungu . ” ( Miyambo 19 : 11 ; Mlaliki 7 : 9 ) Conco ngati munthu wina wakamba kapena wacita cinacake cimene cakukhumudwitsani , muzidzifunsa kuti : ‘ Kodi ndiyenela kumangoganizila za cocitika cimeneci kapena ndiiŵaleko cabe ? ’ Nanga pamakhala zotsatilapo zotani tikatelo ? Ndipo cikumbumtima cotelo cidzatithandiza kupanga zosankha mwanzelu . ( Salimo 119 : 1 ) Manje tiyeni tikambilane mmene tingapezele njila yotithandiza kupeza cimwemwe . Sitepu yoyamba ni kuseŵenzetsa luso la kulingalila limene Mulungu anakupatsa . Musaiŵale kuti ciliconse cimene timacita kuti tikhalebe okhulupilika kwa Yehova cili na phindu lake . Tingatengele bwanji citsanzo ca Paulo ? Komanso ngakhale wolamulila wakhalidwe labwino kwambili amakhala wosadalilika kwenikweni cifukwa ndi wopanda ungwilo . Komabe zimenezi sizitanthauza kuti Mulungu amatiyesa . Mmene Yehova Amayandikila kwa Ife , 8 / 15 Yesu anakambilatu za nthawi yovuta imeneyi , ndipo anatsimikizila otsatila ake kuti adzalandila cilimbikitso kuti akapilile mpaka mapeto . Ndipo ena anali kuyambitsa maganizo opotoka . Hagara anabeleka mwana dzina lake Isimaeli , ndiyeno panapita zaka zambili . Onani njila ziŵili mmene Yehova wacitila zimenezo . Masiku ano , timaonetsa kuti tikucilikiza Ufumu wa Mulungu mwa kuthandiza abale a Yesu ali padziko lapansi pa nchito yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu padziko lonse . — Mat . Pokhala “ womuyenelela ” wa Adamu , mkaziyo anali ‘ wom’thandiza ’ wake . Mwa ici , onse aŵili anabweletsa cimwemwe m’banja tsiku ndi tsiku pocita mbali zawo monga mwamuna ndi mkazi . ( Gen . Kwa io Mau a Mulungu ndi amphamvu . ” — Anatelo Benjamin Cherayath , Papa wa chalichi ca katolika m’nyuzipepala ya Münsterländische Volkszeitung ya ku Germany Iwo anamwalila nili na zaka 14 . Ndiponso zina zimene angapemphe sizikhala zabwino kwa iye ndiponso kwa anthu ena . Tiyeni tikambilane zimene zinacitika ndiponso zimene tingaphunzilepo . Olo kuti poyamba anacita mantha , iye anapempha a tica kuti amulole kufotokoza zoona pa nkhani ya zimene timakhulupilila . A ticawo anamulola . Mofanana ndi akaidi , anthu mamiliyoni ambili amakhala mwamantha cifukwa cokhulupilila zamatsenga na kuopa mizimu yoipa . Zimene timaphunzila zimatithandiza kukonda Yehova ndi kum’lemekeza kwambili . Titam’pempha kukambako mau otsiliza okhudza zaka zambili zimene wakhala mu utumiki wa Yehova , M’bale Franz anati : “ Cimene ningakuuzeni ni ici : Khalanibe m’gulu la Yehova looneka ndi maso zivute zitani . Iye anawalonjeza kuti : “ Ndikuvumbitsilani mkate kucokela kumwamba . ” Mwaŵelama ndi kudoba ndipo mukukondwela kwambili kudziŵa kuti mwapeza golide . Panthawi ya cisautso cacikulu , odzozedwa okhulupilika sadzathandizanso aliyense wosakhulupilika . Zikuoneka kuti Ebedimeleki anali ndi udindo waukulu cifukwa anali kulankhula mwacindunji ndi Mfumu Zedekiya . Koma bwanji ngati tacita chimo lalikulu ? “ Yehova Mulungu Wathu Ndi Yehova Mmodzi , ” June Mwacitsanzo , Mfumu Davide atacita cigololo ndi Batiseba , anapempha Yehova kuti : “ Lengani mtima wolungama mkati mwanga , ndipo ikani maganizo atsopano ndi okhazikika mwa ine . ” Eliya ndi Elisa anayesetsa kuthandiza Aisiraeli mwakuuzimu . Anapeleka moni kwa ‘ wokondedwa wake Epeneto , ’ ndiponso “ Turufena ndi Turufosa , akazi ogwila nchito mwakhama potumikila Ambuye . ” Ngati ife eni sitiphunzila Baibulo patokha , sitingakwanitse kuthandiza anthu amene timaphunzila nawo Baibulo kuona ubwino wocita phunzilo laumwini . Iye amalamulila mwacilungamo . Ndi ulosi wolembedwa pa Danieli 7 : 13 , 14 . Nanga bwanji amai ake ndi agogo ake ? Pambuyo pomvetsela nkhani , mwina munanenapo kuti : “ Nkhani imeneyi monga kuti analembela ine ! ” ( 1 Yohane 3 : 4 ) Ndipo cilango ca ucimo ni imfa , monga mmene Mulungu anauzila Adamu . N’ciani cingatithandize kuona Mulungu tikakumana ndi mavuto ? Komabe , anthu ambili m’nthawi ya Yesu anali kulumbila mwacisawawa . Iwo anali kucita zimenezo n’colinga cakuti anthu ena akhulupilile zokamba zawo . Izi n’zimene zinacitikila Mose . Tinali kukhala m’nyumba ina ya alendo poyembekeza kuti tipatsidwe cilolezo cokhala m’dzikolo . Komabe , tiyenela kucita zimenezo na zolinga zabwino , osati zadyela . 5 : 43 - 48 . Koma mukauwoka , posakhalitsa umayamba kumela mizu ina . Yesaya analosela kuti : “ Anthu ocokela m’mitundu yosiyanasiyana adzabwela n’kunena kuti : ‘ Bwelani anthu inu . Ndiponso “ Yehova anapitiliza kuwaonjezela anthu amene anali kuwapulumutsa . ” Mwacitsanzo , pamene mwamuna wa mlongo Alganesh anamwalila , iye ndi ana ake 6 aang’ono , anathaŵa m’dziko la Eritrea cifukwa ca cizunzo . Kodi tiyenela kupewa ciani ? Federico anati : “ Antonio atasamukila mumpingo wathu , tinayamba kugwilizana kwambili . Kodi ena amene amaoneka ofooka ndi “ olemela m’cikhulupililo ” motani ? Kuukitsidwa kwa Lazalo ndi ena amene analembedwa m’Baibulo kumasonyeza zimene zidzacitika mtsogolo m’dziko latsopano . Onani kuti Paulo anagwilitsila nchito liu la Ciaramu lakuti “ Abba ” limene limatanthauza “ Bambo anga . ” Ndipo cimakhudza bwanji ciyembekezo canu na ubale wanu ndi iye ? * Iwo anali atapanga mzindawu kukhala mudzi wawo . Wandipatsanso anzanga enieni amene ndi amuna ndi akazi Acikristu . N’zoonekelatu kuti aliyense wa ise afunika kukhala woleza mtima ndi wokonzeka kuyembekezela . 3 : 2 , 5 ) Tisapangitse kuti cikhale covuta kwa Akhiristu anzathu kutsatila uphungu umenewu , makamaka ena amene kale anali ndi khalidwe lacisembwele . Ngakhale anthu amene amatizonda amavomeleza zimenezi . Kodi akulu - akulu a boma anacita bwanji poona kaimidwe ka Ophunzila Baibo ka m’Malemba pankhani yomenya nkhondo ? Kodi mitu ya mabanja ili na udindo uti wa m’Malemba ? 13 : 2 ) Yesu anaonetsa kuti kukonda Mulungu n’kofunika kwambili pamene anayankha funso lakuti : “ Kodi lamulo lalikulu kwambili m’Cilamulo ndi liti ? ” ( Mat . Ŵelengani Mateyu 6 : 33 . * Baibulo siinawole ngakhale kuti inalembedwa pa zinthu zosalimba , ndipo inatetezeka kwa anthu otsutsa ndi kwa omasulila amene anafuna kusintha uthenga wake . Iye anati kuganizila lemba la 1 Petulo 5 : 8 kunamuthandiza kwambili . Ndipo okhulupilika amene anabwela ndi Petulo , amene anali odulidwa anadabwa , cifukwa mphatso yaulele ya mzimu woyela inalinso kuthilidwa pa anthu a mitundu ina . ” ( Mac . N’cifukwa ciani anthu a Mulungu ndi ogwilizana ? Mwacitsanzo , tsiku lina mosadziŵa ndinafika pakhomo la munthu wacikulile amene anali kutsutsa coonadi . Pokhala wongocotsedwa kumene m’ndende , n’nali n’kandalama kocepa . ( a ) Kuti Adamu ndi Hava adalitsidwe ndi Mulungu , anayenela kucitanji ? Ise tonse tingalimbikitsane wina na mnzake ( Onani palagilafu 18 ) Linda nayenso anakamba cimodzi - modzi . Pamene mkaziyo anamukakamiza kuti agone naye , Yosefe anakana mosazengeleza . ( Mat . 26 : 39 , 42 ) Yesu “ anapilila mtengo wozunzikilapo , ” ndipo “ sanasamale kuti zocititsa manyazi zimucitikila . ” Nkhani zambili ndi mavidiyo amene ali pa webusaiti yathu amakonzela anthu amene si Mboni za Yehova . Mtumwi Paulo analemba kuti Yehova anapatsa mbali za thupi zosalemekezeka kwambili “ ulemu woculuka . ” ( 1 Akor . ( Luka 4 : 18 , 43 ) Anathandizanso anthu kuona kufunika kosakhala “ mbali ya dzikoli , ” limene silimayamikila zinthu zakuuzimu . — Yoh . 4 : 14 ; Mac . 20 : 5 – 21 : 18 . Lemba la Miyambo 13 : 20 limatiuza kuti : “ Munthu woyenda ndi anthu anzelu adzakhala wanzelu , koma wocita zinthu ndi anthu opusa adzapeza mavuto . ” M’Malemba Acigiriki Acikhristu , timaŵelengamo za anthu ena amene Mulungu anawaukitsa kupitila mwa atumiki ake . 3 Njilayo ‘ Anali Kuidziŵa ’ Ngakhale zili conco , mungafunse kuti : ‘ Kodi Mulungu amandiyang’anila bwanji ? Pofika pano , taona kuti Akhiristu oona analoŵa mu ukapolo m’Babulo Wamkulu pamene atumwi onse anafa . Zocita zathu zoonetsa cifundo . Limatithandiza kumvetsetsa coonadi ca m’Baibulo . Zimenezi n’zogwilizana ndi zimene Baibulo limanena . Baibo imayankha kuti : “ Ndiye cifukwa cake monga mmene ucimo unalowela m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi , ndi imfa kudzela mwa ucimo , imfayo n’kufalikila kwa anthu onse cifukwa onse anacimwa . ” Komabe , m’kupita kwa nthawi , nkhani zina za mu Nsanja ya Mlonda , zinakamba kuti Yesu akanati adziponye pansi kucokela pamwamba pa kacisi , akanafa . ( Yeremiya 8 : 9 ) Zotsatilapo zake zinali zakuti , Yerusalemu anakhala “ mzinda umene uli ndi mlandu wa magazi ” wodzaza “ zinthu zonyansa . ” N’cifukwa ciani inu acinyamata muyenela kutumikila Yehova mokwanila tsopano ? Nthawi ndi nthawi , anali kubwelelanso kukalambila mafano opangidwa ndi anthu . Ngakhale masiku ano , ambili amagwila nchito mwakhama mwakucita mautumiki anthawi zonse osiyanasiyana . Uthenga wa m’Baibulo uli ndi mphamvu kuposa ciliconse cimene tingakambe kuti tifike munthu pamtima . ( Gen . 5 : 29 ; 8 : 21 ) Masiku anonso , ana amene amalambila Mulungu angalimbikitse ena m’banja . Angawathandize kupilila ziyeso zimene akumana nazo masiku ano ndi ziyeso zina zazikulu mtsogolo . Tonse anayi tinatumikila pamodzi kwa zaka zoposa 50 . Koma cocitika cimeneco cidzacititsa mantha anthu a m’dzikoli amene sanamvele cenjezo lakuti afunika kugonjela ku ulamulilo wa Mfumu . Ni makhalidwe ati amene mufunika kupewa kuti musakhale dothi louma limene silingaumbike ? Buku la masamba 128 la Uthenga Wabwino wa Mateyu n’lapadela , ndipo linasindikizidwa kucoka ku Baibulo la Dziko Latsopano m’Cijapanizi . Kapolo ameneyo anali kudzakhala kagulu ka amuna odzozedwa amene anali kudzatsogolela otsatila a Kristu m’masiku otsiliza . 7 , 8 . ( a ) Kodi kusankhana mitundu n’kutani ? Ngati muli na mwana wocotsedwa , kodi mudzakhulupilila Yehova na mtima wanu wonse , na kupewa kudalila luso lanu lomvetsa zinthu ? ( Miy . Ndipo anthu amene amatengela maganizo a Satana angaticititse kuganiza kuti ndife osafunika kwa Mulungu , monga mmene Elifazi wopanda cikhulupililo ananenela . Lemba la Oweruza caputala 6 limanena kuti mngelo wa Yehova anaonekela kwa Gidiyoni ku Ofira . Mwacitsanzo , anawaphunzitsa kuti kusunga mkwiyo kungasonkhezele munthu kucita ciwawa , ndipo cilakolako coipa cingapangitse munthu kucita ciwelewele . ( Mat . Naimwe mungapemphe Mulungu kuti akupatseni mzimu woyela . — Luka 11 : 13 . Patapita zaka 13 , tsiku lina pamene Katharina anali mu Nyumba ya Ufumu na banja lake , anadabwa kuona kuti Hans ndi amene anaitaniwa na cheyamani monga mlendo wodzakamba nkhani . Ndipo Manda anali kumutsatila pafupi kwambili . Kodi ophunzila a Yesu anadziŵa bwanji kuti iye anali kuwakonda ? Simuyenela kungomuuza zimene afunika kucita koma muyenela kumuuzanso cifukwa cake ayenela kucita zimenezo . 22 : 29 , 30 ; Maliko 12 : 24 , 25 ; Luka 20 : 34 - 36 ) Ngakhale kuti sitingakambe motsimikiza , kodi n’zotheka kuti Yesu anali kukamba za ciukililo ca kumwamba ? Maofesi a nthambi m’maiko ena anacitanso cimodzi - modzi . Kumbukilani kuti Mulungu anauza Abulahamu kuti amvele zimene mkazi wake anakamba . ( Gen . Umenewu ndiwo ‘ uthenga wabwino wa Ufumu ’ umene timalalikila “ padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse . ” ( Mat . Ine n’naloledwa kumuthandiza kusamalila pa nyumba imodzi n’colinga cakuti azitsiliza mwamsanga nchitoyo . Kodi tingapewe bwanji ciwelewele ? Mwacitsanzo , kodi panali colakwika ciliconse ndi mmene Mulungu anapangila anthu ? Pambuyo polandila cakudyaco , Lana anayankha mafunso ambili a m’Baibulo ndipo anatenga adilesi , nambala ya foni , ndi imelo yao ndi colinga cakuti azikambilana nao popeza anali ataonetsa cidwi . Ngati ‘ mukuyesetsa kuti mukhale woyang’anila , ’ onetsetsani kuti mukukwanilitsa ziyeneletso zimenezi mmene mungathele . Mu 1959 , n’nalandila kalata yonidziŵitsa kuti n’naitanidwa kukatumikila pa ofesi ya nthambi . Muziika Maganizo Anu pa Nkhani Yaikulu , June 5 : 16 ) Tsopano tikambilana zinthu zitatu zimene zingatithandize kulimbana ndi zilakolako zoipa . Zinthu zimenezi ndi ubwenzi wathu ndi Yehova , malangizo a m’Baibulo , ndi thandizo la Akristu anzathu . Anali kunicitila nkhanza na kuninena , ndipo cinali kuniŵaŵa ngako . Kodi Yesu anaonetsa ciani pamene anasandutsa madzi kukhala vinyo pa phwando la ukwati ? ( 2 Timoteyo 3 : 16 ) Iwo akhulupilila kuti Baibulo lapulumuka cifukwa ni Mau a Mulungu , ndi kuti Iye ndiye waiteteza kufikila masiku ano . Anayesa mobwelezabweleza koma analephela . Kumeneko anapatsidwa mankhwala a anthu amisala . Hans Hölterhoff nayenso anakana kuloŵa usilikali , ndipo anaikidwa m’ndende . Mwacitsanzo , pa Intaneti , pa TV , m’mafilimu , m’mabuku ndi m’magazini amaonetsa kuti ciwawa ndi ciwelewele n’zabwino . Conco musacite mantha : Ndinu ofunika kwambili kuposa mpheta zoculuka . ” — Mateyu 10 : 29 - 31 . Cifukwa cakuti iye amadziŵa bwino zimene anthu ake amafunikila . Ngati tiyesetsa kucita zinthu mogwilizana na zimene timaphunzitsa , tidzakhala otetezeka ku misampha ya Satana . — 1 Yoh . Kunagwa cimvula cacikulu ndipo madzi anadzala ponseponse mofulumila , cakuti magaleta ao sanathenso kuyenda cifukwa anali kumila m’matope . — Oweruza 4 : 14 , 15 ; 5 : 4 . Nchito yao imacilikizidwa ndi zopeleka zimene anthu amapeleka mwakufuna kwao . Ngakhale kuti tinali kusiyana ndi zaka zambili , tinali kusangalala kucitila pamodzi utumiki . 12 : 6 . Anali aakulu ndi olemela makilogilamu 4.5 . 21 : 4 . Ana angapewe kutengela khalidwe losamvela makolo mwa kuganizila zabwino zimene makolo awo amawacitila . ya April 2009 , m’nkhani yakuti “ Zimene Achinyamata Amadzifunsa . . . N’cifukwa ciani kudzikonda pa mlingo woyenelela si kulakwa ? Mnyamata wina wa zaka 20 , dzina lake Bo , anati : “ N’nali kuyopa kulalikila anzanga a m’kilasi . Kodi khama lake linabweletsa mapindu anji ? “ Tamvela , ndikufuna ndikulankhule . ” — YOBU 42 : 4 . Kuwonjezela pamenepo , tiyenela kucita zimene tingathe kuti pakati pathu pakhalebe mtendele ndi mgwilizano . Palinso zifukwa zina zingapangitse munthu kucita zinthu modzikuza . 89 : 34 - 37 ) Zoonadi , ulamulilo wa Mesiya sudzaipitsidwa , ndipo zimene udzacita zidzakhala kwamuyaya ! Kodi mungakonde kuti tidzakambilane nkhaniyi ndikadzabwelanso ? Komabe , sayenela kuiŵala colinga cawo , cimene ni kuthandiza ana awo kukhala ophunzila a Khristu . M’bale wina wa zaka 90 , dzina lake Ionash , anati : “ Gawo la mpingo wathu n’locepa ngako cakuti wofalitsa mmodzi amagaŵilidwa nyumba ziŵili cabe zolalikilamo . Ngakhale n’conco , si kulakwa kuyamikila Wamphamvuyonse pa thandizo limene amapeleka . — Akolose 3 : 15 ; Yakobo 1 : 17 , 18 . Eliezere anapitiliza kuuza amene anamulandila kuti , atafika pa citsime pafupi ndi Harana , anapemphela kwa Yehova Mulungu . Kodi imwe mumakonda kutamba zosangalatsa zabwanji ? Ndi mfundo zotani zimene zimapezeka m’buku la Levitiko ? ( b ) Kodi mungapeleke umboni wotani wosonyeza kuti Ufumu unakhazikitsidwa mu 1914 ? Ufumu wanu ubwele . Posacedwa , mu Ulamulilo wa Khristu wa Zaka 1,000 , iwo adzaponyedwa ku phompho , kumene sadzakhalanso na mphamvu zocita ciliconse . Ndiyeno , masana ndinali kucita nao mapemphelo a Ciyuda ku sukulu . Yohane asanalembe za okana Kristu , Yesu anacenjeza otsatila ake kuti : “ Cenjelani ndi aneneli onyenga amene amabwela kwa inu atavala ngati nkhosa , koma mkati mwao ali mimbulu yolusa . ” ( Luka 20 : 38 ; Aheberi 11 : 17 - 19 ) Mkazi wake atamwalila , Yakobo anali kukonda kwambili ana ake aamuna aŵili amene Rakele anamubelekela . — Genesis 35 : 18 - 20 ; 37 : 3 ; 44 : 27 - 29 . Aisiraeli anabala zipatso zoola cifukwa analeka kulambila Yehova moyenelela . Iwo sanapitilize kukhala mboni zake , m’malo mwake anayamba kulambila mafano . Ni mwayi waukulu ngako kulambila Mulungu , amene anatilenga m’cifanizilo cake . Iwo ananenanso kuti “ maboma sacita khama kuti athetse ziphuphu . ” N’ciani cingakuthandizeni kupilila ? Sikuti nthawi zonse nifunika kucita zinthu zazikulu , nthawi zina ngakhale m’zocita zing’ono - zing’ono ningamuonetse ulemu weni - weni . ” — Megan . Iwo analola kusonkhezeledwa ndi mitundu imene inali kulambila milungu yopangidwa ndi mitengo ndi miyala . Ngakhale kuti Yesu anadabwitsa omvela ake ndi “ mau ogwila mtima , ” iye analemekeza Mphunzitsi wake , Yehova . Ofufuza amakamba kuti : “ M’buku la 2 Samueli sanagwilitsile nchito dzina lakuti Esibaala cifukwa linali kukumbutsa Aisiraeli za mulungu wamvula wa Akanani wochedwa Baala . Koma dzina limeneli . . . lipezekabe m’Buku la Mbiri . ” Kumaphatikizapo mmene timaonela ciyeso ndiponso mmene timamvelela tikakumana ndi mavuto . Tsiku ndi tsiku mkaziyo anali kumupempha kuti akhale pambali pake . Ngakhale kuti acibale ndi mabwenzi athu timawakonda , nthawi zina tingawalankhule mau okhumudwitsa . Apa n’navomela pempho limenelo . Izi n’zimene ena amalemba potonthoza anzawo ofedwa : Baibulo limati : “ Ataona mphepo yamkuntho , anacita mantha . ” M’bale Mumba : Tiyeni tionenso lemba la Yohane 3 : 16 . 34 : 8 . Muzipempha Yehova kuti akuthandizeni . Yehova anakwiya kwambili cakuti anafuna kufafaniza mtundu wonse wa Isiraeli . — Eks . Kodi kuukitsidwa kwa Yesu kunasiyana bwanji ndi kuukitsidwa kwa anthu ena ? N’nali kukondwela maningi nikamvela anthu akunisapota . Cifukwa ca cikondi cake cacikulu , Yehova mofunitsitsa anatilipilila cithandizo ca “ mankhwala ” cimene tinali kufunikila kuti tipulumuke . Tiyeni titengelepo phunzilo pa citsanzo coipa cimeneci . Tiicengete bwino mphatso yathu ya ufulu wosankha zocita , mwa kukangamila kwa Yehova , ndi kuyendela mfundo zake zolungama . — 1 Akor . Zokhumudwitsa na mavuto zingafooketsenso cikhulupililo cathu ndi kucititsa cikondi cathu pa Mulungu kuzilala . Onani Utumiki Wathu wa Ufumu , wacingelezi wa April 2010 , “ Bokosi la Mafunso . ” 3 : 18 . Satana amatiyofya ( Onani palagilafu 14 ) Ciletso ca boma , Kutunthiwa na anzathu a kusukulu , Kutsutsidwa ndi a m’banja lathu 5 : 29 . ( Yoh . 16 : 33 ) Anapitilizabe kulalikila ngakhale kuti anthu anali kumutsutsa . Nanga bwanji za acinyamata amene akuyendabe m’coonadi ngakhale kuti amayetsedwa ndi mayanjano oipa kusukulu ? Tsiku limeneli liyenela kuti linali losaiwalika kwa Yosefe . Iye anati : “ N’napemphela kwa Yehova kuti anithandize kukwanilitsa colinga canga cokukila ku dela la anthu okamba Citandiroyi . ” ( Akol . 1 : 15 ) Ngakhale poyamba Yesu ali kumwamba , anasankha kukhala wokhulupilika kwa Atate wake , ndi kukana kugwilizana ndi cipanduko ca Satana . Popeza tikuyembekezela zinthu zosangalatsa , n’ciani cimene aliyense wa ife ayenela kucita ? Kusankha munthu wokwatilana naye . Mtumwi Yohane analemba kuti : “ Ndinaona mngelo winanso akuuluka capafupi m’mlengalenga . Kodi anthuwo akuzunzidwa kwamuyaya ? Ndithu alimbikitseni , akutelo Mulungu wanu anthu inu . ” — Yesaya 40 : 1 . ( 2 Atesalonika 3 : 2 ) Malemba aŵiliwa atithandiza kuona kuti kulimbitsa cikhulupililo cathu n’kofunika kwambili . Ngakhale n’telo masiku ano pali Mboni za Yehova zokwanila 8 miliyoni zimene zikutumikila Yehova . Iwo amapemphela kuti cifunilo ca Mulungu cicitike pa dziko lapansi , ndiponso amacita cifunilo ca Mulungu . Nthawi zambili munthu amayamba kucita ciwelewele cifukwa ca zimene amaona . Masiku ano , mzimu wa Mulungu umathandizanso Akristu oona kumvetsetsa Baibulo , “ ngakhale zinthu zozama za Mulungu . ” — 2 Pet . ( Yes . 8 : 13 ) Dzina leni - leni la Yesu limatanthauza kuti “ Yehova Ni Cipulumutso . ” mu ulaliki wa kunyumba ndi nyumba pacilumba ca Bali , ndipo alandilidwa mogwilizana ndi cikhalidwe ca ku Indonesia Pamene anali kukamba za Khalidwe limeneli , iye anali kufotokoza za mmene tiyenela kucitila ndi anthu onse ngakhale adani athu . ( 1 Atesalonika 2 : 10 , 11 ) Koma koposa zonse , tiyenela kukhala wokhulupilika kwa Yehova . 7 : 12 ; Akol . Komanso analimbitsa “ kwambili ” citetezo m’mizinda ina . Kumatanthauza kukondesetsa zinthu zakuthupi kuposa zinthu za kuuzimu . Muzipeza nthawi yoceza ndi ana anu , kudya nao , kuseŵela nao , kapena kuwakumbatila . “ Ine [ mneneli Danieli ] ndinapitiliza kuyang’ana kufikila pamene mipando yacifumu inaikidwa ndipo Wamasiku Ambili [ Yehova ] anakhala pa mpando wake wacifumu . . . . Baibulo imapeleka zifukwa zabwino zimene aŵiliwo safunikila kulekana . Mwa kuphunzila ndi kucita zimene Mulungu amafuna kwa inu . * Nanga tingacitepo ciani pa mphatso imeneyi ? Mwacitsanzo , mlongo wina amene anali mmishonale mu Africa muno yemwe anabatizidwa mu 1948 anakamba kuti : “ Mogwilizana ndi pemphelo lacitsanzo limeneli , ndimapemphela kuti anthu onse amene ali ngati nkhosa athandizidwe kudziŵa Yehova nthawi isanathe . Pano pamene tikamba , iwo akuthandiza pa nchito yomanga ofesi ya nthambi m’dziko la Micronesia . Ndi bwino kukhala monga mtumiki wa Yehova , Davide , amene anathaŵa cifukwa ca nsanje ya Mfumu Sauli . Tinalembela ku ofesi ya nthambi kufunsa ngati kuli malo osoŵa kumene tingapite kukathandiza . Tiyeni tione cifukwa cake yankho lake ndi lakuti inde . Iye anayamba kukambilana ndi mai wina amene anabwela kudzatunga madzi pa citsimepo . N’zimenenso Atate wathu Yehova amacita . Makhalidwe amenewa amasiyanitsa kwambili anthu na zamoyo zina zonse padziko lapansi . Pamene m’busa anauza Msulami kuti apite limodzi kokayenda , azilongosi ake anamuletsa . Koma , kunyumba imeneyi , ndinayamba kuona kuti sindidzakwanitsa kucita zonse zimene ndinali kufuna . Kumbuyoku , tinafotokoza kuti anthu a Mulungu anakhala akapolo a Babulo Wamkulu kwa kanthawi kocepa kuyambila mu 1918 . Yehova anaona kuti tinali ofunitsitsa kucita zambili mu utumiki , conco anatitsegulila “ zipata za kumwamba ” ndi kutikhuthulila madalitso . ( Mal . Iwo anapeza nchito kuti azipeza zofunikila paumoyo wawo pocita upainiya . Ndipo lomba atumikila mumpingo wina m’cigawo ca Veraguas , m’dziko la Panama . Nawonso ophunzila aŵili amene anakumana ndi Yesu panjila yopita ku Emau , pambuyo pakuti waukitsidwa , anaona kuti zinthu zina zokhudza Mesiya zimene anali kuyembekezela sizinakwanilitsike . ( Ŵelengani Yakobo 4 : 17 . ) Zimene anayankha zinaonetsa kuti iye anali kudziŵa kuti zilizonse zimene Yehova angam’pemphe kucita , ndi zabwino . Zitanthauza kuti maganizo athu ayenela kukhala oyela , ndipo tiyenela kuleka kucita ciliconse coipa . Kukambilana ndi ana anu kaŵilikaŵili , kudzakuthandizani kudziŵa maganizo ao ndi zimene afuna . Ayuda oukila anasangalala , ndipo anathamangila asilikali amenewo . N’ciani cimene Yesu anacita usiku wa pa Nisani 14 , mu 33 C.E . ? Citsanzo cina ca m’Baibo pa nkhani ya kudziletsa ni ca Mfumu Davide . Iye anafuna kuti anthuwo akhale ndi moyo kosatha , adzaze dziko ndi kulisandutsa kukhala paladaiso . ​ — Ŵelengani Genesis 1 : ​ 28 , 31 . Anam’dalitsa Yesu m’njila imene iye sanali kuyembekezela . Anamuukitsa n’kumuika “ pamalo apamwamba ” ndipo anamupatsa cinthu cimene aliyense anali asanalandilepo . Anamupatsa moyo wosafa . * ( Afil . 2 : 9 ; 1 Tim . 6 : 16 ) Zoonadi ! Conco , Yesu adzaukitsa wocita zoipa wosalungama uja amene anakamba naye , pamodzi ndi anthu ena mamiliyoni , ngakhale mabiliyoni , amene anafa osadziŵa cifunilo Mulungu . Lefèvre d’Étaples — Anafuna Kuti Anthu Wamba Adziŵe Mau a Mulungu 10 Lonjezo limene Danieli anapatsiwa , komanso yankho loonetsa cikhulupililo limene Marita anapeleka pamene anali kukamba na Yesu , ziyenela kulimbitsa cikhulupililo cathu cakuti akufa adzauka . Ena mwa iwo anali Abele , Inoki , Nowa na banja lake . Akatswili ofufuza malo amakamba kuti anapeza malo amene panali paradaiso wakale . Mwacitsanzo , Charles Gordon , mkulu wa asilikali a Britain , anayendela dziko la Seychelles mu 1881 . Iye anacita cidwi kwambili ataona malo ena okongola m’dzikomo ochedwa Vallée de Mai , amene tsopano ni malo a zacilengedwe ofunika kwambili padziko lonse . Anakamba kuti malowo ni munda wa Edeni . Ngati n’conco , onani zimene tingaphunzile pa nkhani ya Mose . Iye anali kufunitsitsa kulalikila anthu okamba Cirasha amene anasamukila m’dzikolo . Kodi boma la padziko lonse lingagwilizanitse bwanji anthu a mitundu yonse ? Kafukufuku wina anaonetsa kuti ngakhale anthu amene sapita ku chalichi , amapemphela nthawi zonse . ( Malinga ndi buku yakuti Faith on the March yolembewa na A . Sauli anali cabe ndi asilikali 600 , ndipo iye ndi Yonatani ndiwo okha amene anali ndi zida za nkhondo . Poganiza zinthu ngati zimenezi , anthu ena amacita mantha , ena amakayikila , ndipo ena zimawaseketsa . Olo kuti anali wotangwanika kwambili , anayamba kuphunzila Baibo . Kuphedwa kwa Ahabu kunakumbutsa Eliya , Elisa ndi anthu ena a Mulungu okhululupilika kuti Yehova sanaiwale kulimba mtima ndi cikhulupililo ca Naboti . Ngakhale n’conco , tingafunse kuti : ‘ Kodi inu mudzakopeka na bodza limenelo ? ’ Tikamatelo , tidzasonyeza kuti tikumvetsetsa tanthauzo la mau a Yesu . Amishonale oposa 8,500 amene analoŵa Sukulu ya Gileadi atumizidwa m’maiko 170 kuyambila mu 1943 Cifukwa cofunitsitsa kukondweletsa Yehova ndi kukhalabe mumpingo wacikristu , atumiki ambili a Mulungu amagwilitsila nchito malangizo acikondi amene apatsidwa . — Yak . * Banjalo linadzimva monga kuti mkambi akukamba ndi io mwacindunji . Kodi Aisiraeli anakhala na maganizo anji odzinamiza ? Nanga Yehova anamvela bwanji cifukwa ca zocita zawo ? Ngakhale n’conco , zolakwa zimacepa ngati tiganizila mfundo zofunika kwambili za m’Malemba . N’zinthu zina ziti zimene timacita mwacibadwa , zimene zimatipatsa cimwemwe ? Patapita nthawi , ine ndi Aarhonda tinaloŵa Sukulu ya Gileadi Yophunzitsa Baibulo ndipo pambuyo pake tinauzidwa kuti tikatumikile ku Panama , kumene tinapitiliza kutumikila monga amishonale . M’kupita kwa nthawi , thupi la Elisa linawonongeka n’kukhala mafupa okha - okha . N’zoona kuti m’kupita kwa nthawi zinthu zikhoza kusintha paumoyo wathu . Koma Mkulu wa Angelo anadziŵa kuti mphamvu zake zili ndi polekezela . ( a ) N’cifukwa ciani tiyenela kupeleka mapemphelo aciyamiko ? Kulanga ana tingakuyelekezele ndi kusamalila maluŵa . Mu 1881 ku Praslin , Seychelles kumene Gordon , mkulu wa asilikali , anaona kuti wapeza munda wa Edeni N’nazindikila kuti kupanda cilungamo kunali kofala m’dziko la GDR . Kuyamikila Yehova ndi kum’konda , kwanithandiza kuti nileke kucita zankhanza . ” Boma la dziko limeneli linati anthu oposa 300 sauzande anafa . Komabe , nthawi zina tingavutike kwa nthawi yaitali . Misonkhano imatiphunzitsa kuti tizicita zimene timaphunzila m’Baibulo . Iye anawononga cuma cake conse koma . . . matendawo ankangokulilakulila . ” Mipingo ina yapindula kukhala ndi apainiya apadela . Mwacitsanzo , ngati munthu amene mumam’konda anamwalila kapena ngati mudwala matenda osacilitsika , palibe mocitila koma kungopeza njila zokuthandizani kupilila . Abusawo akaona anthu akuseŵenzetsa mabuku ena a m’Baibulo , kusiyapo buku la Masalimo la Cilatini , anali kuwaona ngati ampatuko . Atsogoleli a chalichi cina analamula amuna ena kuti ‘ akafufuze mwakhama anthu ampatuko m’nyumba zonse zimene anali kuganizila kuti muli Mabaibulo . . . . Yesu anawadzudzula Ayuda cifukwa cotenga malumbilo mopepuka . Anzanga ambili amene ndinali nao ndi olemela koma alibe cimwemwe . Patapita nthawi , Paulo analemba za Timoteyo kuti : “ Ndilibe wina wamtima ngati iye , amene angasamaledi za inu moona mtima . ” Iye anali kufunafuna anthu amene anali kufunika thandizo . Kodi kulalikila mogwila mtima kumadalila pa ciani makamaka ? Wophunzila ni munthu amene waphunzila na kumvetsetsa ziphunzitso za Yesu , ndipo ni wokonzeka kucita zimene waphunzilazo . Ngati tisinkhasinkha za cikondi cacikulu ca Yehova pa ife ndi mmene amacionetsela , timam’yandikila ndi kum’konda kwambili . Baibo ili na matanthauzo osiyana - siyana pa liu lakuti “ thupi . ” N’cifukwa ciani makolo ndi ana ayenela kukambitsilana pasadakhale za kumene makolo adzakhala akadzakalamba ? Yesu anauza ophunzila ake kuti safunika kutengako mbali m’zandale . Zaka pafupifupi 400 Kristu atapita kumwamba , John Chrysostom anakamba kuti ziphunzitso za Yesu zinali zitamasulidwa m’zinenelo za Asuri , Aiguputo , Amwenye , Aperisiya , Aitiyopiya ndi m’zinenelo zina zambili . Mose anali kuopanso kuti anthu a mtundu wake sadzakhulupilila kuti Yehova anam’sankha kuwatsogolela kutuluka mu Iguputo . Mu 71 C.E . , Tito anabwelela ku Italy , ndipo analandilidwa na nzika za Roma mwa cisangalalo cacikulu . Mau a Mulungu amati iye anakhala “ munthu wofatsa kwambili kuposa anthu onse amene anali padziko lapansi . ” kudzakuthandizani bwanji kuti musamaope anthu ? Nkhaniyi idzatithandiza kuona ngati cikhulupililo cathu cayamba kufooka ndi mmene tingacilimbitsile . Conco , ena akatilakwila , tiyeni tiziwacitila cifundo , monga mmene Atate wathu , Yehova , amacitila kwa ife . — Ŵelengani Salimo 103 : 12 - 14 . N’cifukwa ciani tifunika kuyamikila kwambili Mau a Mulungu ? Nsembe ya mikate inali kuimila ophunzila a Yesu amene anadzozedwa . Baibo siikamba cimene cinacititsa Hezekiya kukhala ndi mtima wodzikuza . 3 : 15 ; Aheb . 2 : 10 , 18 ) Conco , tingakhale na cikhulupililo cakuti ngakhale lomba , Khristu amakhudzidwa na mavuto amene timakumana nawo , amamvetsetsa cisoni cimene timakhala naco , ndipo amatipatsa citonthozo “ pa nthawi imene tikufunika thandizo . ” — Ŵelengani Aheberi 4 : 15 , 16 . Anthu amaonetsa cikondi caciphamaso pofuna kupusitsa anzawo . Pamene tikambilana mapangano angapo ochulidwa m’Baibulo , tidzaphunzila mmene amagwilizanilana ndi boma lakumwamba . Tidzaphunzila cifukwa cake tiyenela kukhala ndi cidalilo colimba mu Ufumu . Kodi kupemphela nthawi zonse kungatithandize bwanji kukulitsa cikondi cathu pa Mulungu ? Baibo siilimbikitsa kuti tizingoganizila za mavuto athu kapena zofuna zathu zokha . M’malomwake , imatithandizanso kuzindikila kuti palinso zinthu zina zofunikila kupambana ise . Mutke ) , Na . Yehova watidalitsa pogwila nchito yake m’nthawi zovuta ndi m’nthawi zabwino . 4 : 7 ) Munthu wocita maseŵela othamanga amakhala na kochi , koma amafunikanso kumadziphunzitsa yekha . ▪ ‘ Tsopano Ndinu Anthu a Mulungu ’ 24 : 45 - 47 ; Yoh . 10 : 16 ) Kuyambila mu 1919 , kagulu kocepa ka abale odzodzedwa , mokhulupilika kakhala kakugwila nchito yofunika kwambili yopatsa “ anchito apakhomo ” cakudya cakuuzimu . Tinenenso kuti m’bale wabwela kumisonkhano pambuyo pa miyezi yambili . Iye anati : “ Kukhala tsiku limodzi m’mabwalo anu n’kwabwino kuposa kukhala masiku 1,000 kwina . ” ( Sal . Koma ndife osangalala cifukwa cakuti tikudziŵa mmene Mulungu amaonela khalidwe limeneli . — Ŵelengani Yuda 14 , 15 . Tinali kuganizanso kuti ngati m’machalichi akuluakulu mulibe zinthu zimene tinali kufunafuna , ndiye kuti kagulu ka m’patuko monga ka Mboni za Yehova sikangakhale nazo . ” — Kent wa ku Washington , U.S.A . Makolo ake akamuuza kuti amupatsa cilango cifukwa colakwitsa zina zake , anali kuonetsetsa kuti amupatsadi cilangoco . Cikapeza malo amene pali mphepo yothuma , ciwombankhanga cimatambasula mapiko ake n’kumauluka mozungulila pamalopo mpaka kupita m’mwamba kwambili . N’cifukwa ciani cikondi pakati pa Mulungu ndi Mwana wake cinakula kwambili ? Aliyense wa ife akaona coopsa amabisala kapena kuthawa . Kodi zimene Margaret analakwitsa kuciyambi kwa nkhani ino , zinasokoneza maceza awo a banja ? Kodi kuyamikila acicepele kungakhale ndi zotsatilapo zotani ? Iye anadziŵa kuti Ahabu anali wakuba , wakupha ndi wopandukila Yehova Mulungu . 4 : 13 ) Kukamba zoona , ndise oyamikila ngako kuti mapemphelo athu amayankhidwa , komanso kuti tili na mwayi wokhala pa ubwenzi na Yesu . Mwacitsanzo , Hosa wa ku Brazil wa zaka 85 , amayesetsa kuthandiza ena ngakhale kuti ndi wacikulile . Powakhazika mtima pansi , M’bale Jaracz anati : “ Tsopano tiyeni tipatse mpata mzimu woyela kuti ugwile nchito yake . ” Kodi “ nchito zosonyeza kuti ndinu odzipeleka kwa Mulungu ” n’ciani ? Koma “ cilengedwe conse cikubuula limodzi ndi kumva zoŵaŵa . ” 22 : 21 ) Yesu anali kudziŵa kuti okhometsa msonkho ambili anali acinyengo . Munthu wodzicepetsa asanavomeleze udindo winawake , amayamba waona ngati angaukwanitse bwino - bwino . N’citsanzo canji cimene Yesu anapeleka pa nkhani ya zosangalatsa ? Ndipo Satana amafunitsitsa kuti ulamulilo wa Yehova uthe . Nthawi ya cakudya imapelekanso mpata wabwino wokambilana momasuka . 3 Mau Amene Anali Atanthauzo Kwambili Onani “ Mafunso Ocokera kwa Owerenga ” mu Nsanja ya Olonda ya May 15 , 2002 . Mzindawu unali pa mtunda wa makilomita 1,900 . Munthu wina mumpingo wacikhristu , dzina lake Diotirefe , sanali kufuna kulandila Akhristu oyendela . ( Yesaya 40 : 26 ) Cilengedwe ca Mulungu cimationetsa kuti iye ndi “ Wamphamvuyonse ” — ndi “ wamphamvu zambili . ” — Yobu 37 : 23 . Pounika mbali ya aliyense m’banja , Paulo analemba kuti : “ Akazi agonjele amuna awo ngati mmene amagonjelela Ambuye , cifukwa mwamuna ndiye mutu wa mkazi wake , monganso mmene Khiristu alili mutu wa mpingo . ” ( Aef . Mipingo inatsatila malangizo awo ndipo “ inapitiliza kulimba m’cikhulupililo ndipo ciwelengelo cinapitiliza kuwonjezeka tsiku ndi tsiku . ” N’cifukwa ciani kupeleka ulemu woyenelela kwa akulu n’kofunika ? Tikasinkhasinkha kwambili zinthu za kuuzimu , tidzaziŵanso zinthu zambili zatsopano zokhudza Mulungu wathu , Yehova . Nayenso Claudia , Mkhristu amene ni mbeta , anasamukila kumadela kumene alengezi ni ocepa . 10 , 11 . Ezekiel , amene ali na zaka za m’ma 20 anati : “ Kale , n’nali monga munthu amene ayendetsa motoka koma sadziŵa kumene ayenda . Makolo ake anali osiyana kwambili ndi anthu a ku Harana . Pa nthawi ina iye anati : “ Coonadi cidzakumasulani . ” Kodi cifuno cina cacikulu ca cikwati cinali ciani ? Popeza ndife Mboni za Yehova , Akhiristu anzathu analinso kutithandiza . ( Aheberi 13 : 5 ) Mobwelezabweleza , Yehova anathandiza anthu oona mtima ndipo adzapitiliza kuthandiza amene amakhala oona mtima nthawi zonse . Mu 740 B.C.E . kutatsala zaka zambili kuti Ezekieli alosele , Asuri anagonjetsa ufumu wa Isiraeli wakumpoto ndi kutenga anthu kupita nawo ku ukapolo . ( 2 Maf . ( b ) Kodi Yesu anapeleka malangizo anzelu ati pankhani yokonda cuma ? ( b ) N’ciani cingathandize Akhristu acicepele kukana ngati ayesedwa kucita khalidwe loipa ? Kodi tingadziŵe bwanji zenizeni ? Mukatelo , adzaona kuti mumadalila Yehova , ndipo naonso adzaphunzila kucita cimodzimodzi . 3 : 15 ) Citsanzo ca Petulo cingatithandize kukhala ndi mzimu wodzimana . M’nkhani ino ndi yotsatila , tidzakambilana mafanizo 7 a Yesu . Sitilipilidwa kuti tilalikile , tiphunzitse ena mu mpingo kapena timange malo olambilila . Muyenela kumvela ndi mtima wonse malangizo a m’Baibulo amene angakuthandizeni kupewa chimo ndi kukhalabe oyela . — Ŵelengani Yakobo 1 : 21 - 25 . Mwacitsanzo , m’magazini ino muli lemba la “ Yesaya 40 : 13 , ” limene lionetsa zotsatilazi : Ndiyeno , Yesu anauza anzake fanizo lina . YEHOVA anatilenga ndi maluso apadela . ( Yer . 23 : 26 , 27 ) Zotulukapo zake n’zakuti anthu oona mtima asoceletsedwa , ndipo mosadziŵa amalambila ziŵanda m’malo molambila Mulungu . ( 1 Akor . 10 : 20 ; 2 Akor . Ndipo Yehova amadalitsadi kwambili . ” Ngati iwo akumana ndi mavuto m’cikwati , safunika kufuna - funa njila zosakhala za m’Malemba zothetsela cikwati . Akhristu a m’nthawi ya atumwi , anali citsanzo cabwino pankhani yoimba nyimbo zotamanda Mulungu . Ndiyeno ŵelengani Mateyu 5 : 3 ndi kuyambitsa phunzilo . Popanga zosankha zazikulu , njila imodzi yoonetsela kukhulupilila Mulungu ndiyo kupeza thandizo m’Mau ake ndi gulu lake . Ngati muimba mokweza na mokondwela , mudzalimbikitsanso ena kucita cimodzi - modzi . Ganizilani za Baruki , mlembi wa mneneli Yeremiya . Yehova anaika malamulo a mmene cilengedwe cake ciyenela kugwilila nchito mogwilizana . Anaonetsa kuti amawadalila mwa kuwapatsa malangizo okhudza nchito yofunika kwambili yophunzitsa anthu . Kodi timaonetsa bwanji kuti tifuna kukhalabe m’cikondi ca Khristu ? Imfa ya Naboti sinali kuimila imfa ya Yesu kapena odzozedwa . 8 Cilimikani pa Kulimbana Kuti Mupeze Madalitso a Yehova Pambuyo pakuti woyang’anila dela wacezela mpingo wao maulendo angapo aposacedwapa , akulu anafotokozela Fernando zimene ayenela kucita kuti ayenelele maudindo oonjezeleka mumpingo . Tingam’dziŵe bwanji munthu amene si bwenzi labwino ? Mwacitsanzo , palibe paliponse m’Malemba pamene paonetsa kuti iwo angakwanitse kudziŵa zimene zili m’maganizo kapena mumtima wa munthu . Kodi Yehova amaticenjeza bwanji tikayamba kulakalaka zoipa ? Kuti athandize ophunzila ake , Hutter anaseŵenzetsa njila yaluso yolembela zilembo . Baibulo limati : “ Munthu amaona zooneka ndi maso , koma Yehova amaona mmene mtima ulili . ” MFUNDO YA M’BAIBO : “ Kupuma pang’ono kuli bwino kuposa kugwila nchito mwakhama ndi kuthamangitsa mphepo . ” — Mlaliki 4 : 6 . Akhristu a m’mipingoyo ‘ ataiŵelenga [ kalatayo ] , anakondwela cifukwa ca mau olimbikitsawo . ’ — Mac . 15 : 27 - 32 . Pofotokoza zimene zinamucitikila , onani kuti Yosefe anakamba kuti anacita ‘ kumuba ’ . ( Yoh . 19 : 26 ; 20 : 13 ) Koma panalinso mau ena amene anali ofunika kuposa pamenepa . Iye anaimilila pamalo ena ake kuti akhale pafupi ndi Yesu . 141 : 5 ; Aheb . Ndife otsimikiza mtima kuti ngati titsatila zimene Baibulo limakamba , tikhoza kusamalila zosoŵa za banja lathu . Ndani anaimbidwa mlandu cifukwa ca kucimwa kwa anthu aŵili oyamba ? Conco , “ cizindikilo ” cimene Yesu anapeleka ca kukhalapo kwake kosaoneka monga Mfumu yatsopano ya dziko lapansi cinayamba kukwanilitsidwa . ( Mat . Baibo siikamba mwacindunji tsiku limene Yesu anabadwa . Ena amaganiza kuti pamene Baibo ikamba kuti kumwamba ndi dziko lapansi “ azisungila moto , ” itanthauza kumwamba kweni - kweni ndi dziko lapansi leni - leni . 11 : 28 - 30 ) Mau amenewa ni a zoona . Aisiraeli m’cipululu sanayamikile zimene Yehova anali kuwacitila . Tingatengele bwanji cikhulupililo ndi kumvela kwa Nowa ? ( Luka 4 : 18 ) Kucita zimene Mulungu afuna kunam’cititsa kukhala wacimwemwe . Kodi tiyenela kudzifunsa mafunso ati pankhani yolankhulana ndi Yehova ? Baibo imakamba kuti kukhala na ciyembekezo n’kofunika kwambili , ndipo kumatithandiza kupewa kukhala na ziyembekezo zabodza . N’zomvetsa cisoni kuti ena anaphedwa . ( Salimo 83 : 18 ) Mumpingo munali anthu amitundu yosiyanasiyana , koma pakati pao panalibe tsankho . Tumapepalatu ndi tosavuta kutugwilitsila nchito . Zimatipatsanso mpata woganizila cifukwa cake tinali kutumikila pa maudindo amenewo . 1 : 3 ) Zozizwitsa zimene Yesu anacita zimatsimikizila kuti iye ndi Atate ake amalakalaka kuthetsa matenda ndi imfa . Ngakhale n’conco , iwo amaona zimene timacita . ( Aroma 6 : 23 ) Baibulo limafotokozanso kuti : “ Munthu amene wafa wamasuka ku uchimo wake . ” Popanda mame , zomela zimafota ndi kufa . Akhiristu ku Korinto anayamba kugaŵikana cifukwa ca nkhani ya kudya nyama zimene zinali zopelekedwa nsembe ku mafano , koma pambuyo pake zinali kugulitsidwa pa maliketi . Kwa zaka masauzande ambili , Yehova wakhala akupilila kunyozedwa kwa dzina lake . Anafuna kukwatila mtsikana amene sanali kutumikila Yehova . Ndinakambilana ndi woyang’anila dela Kurt Kuhn , kuti ndimve maganizo ake cifukwa ndinali kufuna kugwila nchito kwa miyezi ingapo kuti ndigule galimoto yocitila upainiya . Mwina amacita zimenezi cifukwa afuna kuti anthu aziwatamanda , ndi kuti akhale oyamba kufalitsa nkhaniyo . Komiti ya Utumiki ya Mpingo iyenela kukuikani m’kagulu ka ulaliki mwamsanga mukangofika . Kupitila m’Mau ake , Yehova amatilangiza mobweleza - bweleza kuti tiziseŵenzetsa bwino maluso athu . Lomba nimakondwela na utumiki wanga . Nimauona kuti ni utumiki wabwino ngako ! ” Onani mbali ziŵili izi . N’cifukwa ciani ngakhale Akhiristu odzozedwa anafunikila kucenjezedwa kuti asakhale na umoyo wotsatila za thupi ? Malangizo a m’mabuku a zamankhwala , amene kale anali kudziŵika kuti ni othandiza , m’kupita kwa nthawi anapezeka kuti ni oopsa . Kodi mumacita zimene mungakwanitse kuti mpingo ukhalebe wogwilizana ? OLOŴETSEDWAMO : Yehova ndi Abulahamu 1 : 19 ) Amakonda anthu kwambili cakuti anali wofunitsitsa kupeleka Mwana wake wobadwa yekha kuti adzatifele . ( 1 Yoh . Kukhala wozindikila kumatanthauza kukhala ndi luntha losiyanitsa cabwino ndi coipa , ndi kusankha njila yabwino . ( Aheb . Mkristu wofikapo amakhala wodzicepetsa , ndipo amatsatila malangizo ndi miyezo ya Yehova osati maganizo ake . Izo zimatsatila miyezo ya m’Baibulo ndi citsanzo cimene Yesu ndi ophunzila ake anapeleka . Conco , tifunika kukhala osamala pankhani ya mankhwala amene angaoneke monga angaticilitse , koma palibe umboni wakuti anacilitsapo munthu . Yehova walonjeza kuti , “ adzamvetsela pemphelo la anthu amene alandidwa ciliconse , ndipo sadzapeputsa pemphelo lao . ” ( Sal . Motelo , tiyeni tipende salimo limeneli mosamala kwambili . TSOGOLO LANU Kodi pali ulosi wodalilika umene umakhudza tsogolo lanu ndi la acibale anu ? Kuti tikhalebe osalakwa m’dziko loipali , tifunika kuphunzitsa ‘ mphamvu zathu za kuzindikila ’ kuti tizikwanitsa kusiyanitsa zoyenela na zosayenela komanso zanzelu na zopanda nzelu . — Aheb . Hava anamvela malangizo amene Satana anapeleka kudzela mwa njoka , ndipo Adamu anamvela mkazi wake . Koma ‘ ambili mwa iwo anali kutsatila [ Yesu ] . ’ 9 : 24 - 26 ) Idzacotselatu ucimo umene tinatengela kwa Adamu . Malonjezo a Mulungu salephela kukwanilitsika . — Yes . Kenako ndinapemphela uku ndikulila . ( Sal . 21 , 22 . ( a ) Kodi lemba loyenelela lingasinthe motani umoyo wa munthu ? 13 : 14 , 45 - 47 ) Kucokela m’nthawi ya atumwi , gulu la Mulungu lakhala likuuza anthu zimene Yehova wacita kuti apulumutse anthu . Kodi tingasoyenze bwanji mzimu wodzimana panthawi yovuta ? Nanga n’cifukwa ciani ? ( b ) N’cifukwa ciani anthu opita ku ubatizo amafunsidwa ngati anadzipeleka kwa Yehova ? Mwina mumayelekezela kuti muli ndi moyo wosatha padziko lapansi . Izi ndi zitsanzo zocepa cabe za anthu amene amacita cinyengo . Zokondweletsa n’zakuti mu 1962 , atate anabatizika n’kukhala Mboni . Yesu anali kukonda kuphunzitsa anthu za Atate wake wakumwamba . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Aliyense akhale wofulumila kumva [ ndi ] wodekha polankhula . ” — Yakobo 1 : 19 . ( b ) Nanga zimene banja lina linacita zionetsa bwanji kuti kutsatila mfundo za m’Baibulo n’kwanzelu ? N’cifukwa ciani kufatsa na kuleza mtima ni makhalidwe ofunika ? Tiyeni tizicita zinthu mozindikila pamene tikuthandiza pa nchito yongokoletsa paladaiso wauzimu . Ndipo analonjeza kuti adzasintha khalidwe lake . ” Yesu anali kukambilana ndi ophunzila ake . Iye anayesetsa kuti akhazikitse mtendele . Kodi mapikica amenewa amaonetsa Yesu molondola ? Anthu akatitamanda , tingacite bwino kutsatila mau a Yesu akuti : “ Mukacita zonse zimene munapatsidwa ngati nchito yanu , muzinena kuti , ‘ Ife ndife akapolo opanda pake . Mosakaikila mudzacoka pamalopo ndi kukafunafuna malo ena . Iye anati : “ N’naona kuti Yehova ananidalitsa panthawi yovuta imeneyo , ndipo ananipatsa mphamvu kuti nikwanitse kucita zinthu zimene zinacititsa kuti dzina lake litamandidwe . ” Kodi tingacite bwanji kuti tizilimbikitsa ena ? N’nayamba kucita upainiya n’tangotsiliza sukulu . Malinga na Cilamulo ca Mose , anthu odwala matenda ena anali kufunika kukhala kwaokha . Pamene Yehova anam’lamula kuti amange cingalawa , Nowa sanadalile luso lake . 2 : 2 ) Kuti tipeze yankho , tiyeni tikambilane citsanzo ca Timoteyo . Iye anali kumvetsetsa mavuto amene anali kukumana nawo kucokela kwa adani awo . ( Mat . 7 : 24 , 25 ) Tiyeni tikambilane mmene citsanzo ca Mfumu Sauli ndi mtumwi Petulo cingatithandizile kukhalabe ndi mzimu wodzimana . Nayenso Lennart wa ku Sweden wa zaka 75 pofuna kuphunzila zinthu , anayamba kuphunzila cinenelo cina . M’malo mwake akufotokoza zocitika za mbali yomaliza ya cisautso cacikulu . ( Chiv . Anthu onse pamsonkhanowo anayankha mokweza kuti : “ Inde ! ” M’malo modalila atsogoleli aumunthu kapena mabungwe olimbikitsa ufulu , Paulo na Akhristu anzake anali kugwila mwakhama nchito yophunzitsa anthu uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . Nthawi zambili amatitsutsa tikawauza kuti dzikoli liwonongedwa posacedwa . Komanso n’nazindikila kuti nyimbo zina zinali kunicititsa kukhala na cilako - lako cofuna kukoka camba . Ngakhale pamene ana akali aang’ono , mungawauze kuti : “ Ukaona ciliconse pa Intaneti cimene cakucititsa kufunitsitsa kuonelela zamalisece , uzindiuza . Nthawi zina ndinali kukwela sitima pokacezela mipingo nditanyamula masutukesi olema . Adamu anadya cipatso cimene analetsedwa . Davide anauza Abigayeli kuti : “ Adalitsike Yehova Mulungu wa Isiraeli , amene wakutumiza kudzakumana nane lelo ! Conco , anapeleka mlandu umenewu kwa Woweluza wa Mkulu , Yehova , amene ali ndi mphamvu zonse zoweluza Satana . ( Machitidwe 10 : 40 , 41 ) N’cifukwa ciani sanaonekele kwa anthu onse ? Kodi kukhala okhulupilika pa mayeselo kuli na phindu lanji ? ( b ) Kodi acicepele ena amadandaula na ciani akakula ? Nanga iwo angalipewe bwanji vuto limeneli ? Cesar ndi Rocio anati : “ Tinaona kuti umenewu ndi mwai wathu wotumikilako pa Beteli , cifukwa tinali titayamba kukalamba . Kunena zoona , ndi mwai wamtengo wapatali kuthandiza Yehova pa nchito yokongoletsa paladaiso wauzimu . Popeza kuti timakonda Mau a Mulungu , timafuna kupindula nawo mokwanila . Yesu anakamba kuti Yehova akhoza kupangitsa miyala kulengeza za Ufumu wa Mulungu ndi Mfumu yake . Tsiku lotsatila , pamene tinacoka m’nyumba tinapeza kuti manyumba ambili awonongeka . Pamene mtendele wa m’maganizo mwake unali kuwonjezeleka , Inoki anagona tulo twa imfa . 5 : 4 - 6 ) Zimenezi zionetsa kuti Yehova iye mwini adzagwilitsila nchito Ufumu wa Mesiya kudalitsa mitundu yonse , ndi kukwanilitsa cifunilo cake coyambilila ca dziko lapansi cokhudza anthu . N’cifukwa ciani citsanzo ca makolo n’cofunika kwambili ? Nanga makolo ena anaonetsa citsanzo canji kwa ana awo ? Kenako , io anayamba kumenyana okhaokha ndi kuphana mpaka Aisiraeli anawina nkhondoyo . — 1 Samueli 13 : 5 , 15 , 22 ; 14 : 1 , 2 , 6 , 14 , 15 , 20 . Anthu ambili masiku ano akusangalala ndi umoyo wabwino umene kale unali kuoneka wosatheka . Tifunika kuwayamikila pa nchito yaikulu imene amacita ndi kuyesetsa kumvela malangizo amene amatipatsa . Paulo analembela Akristu a ku Korinto kuti “ Sitikubwelela m’mbuyo . Kodi izi sizikupangitsani kumuyandikila kwambili Mulungu wathu wacikondi ndi wopanda tsankho ? — Mac . 10 : 34 . Ndipo Mkwati , amenenso ndi Mfumu , adzakhala ndi cimwemwe codzaza tsaya cifukwa cakuti mafumu anzake onse ‘ adzadya ndi kumwa ’ mophiphilitsa pamodzi naye ‘ patebulo lake mu ufumu wake . ’ Nanga n’cifukwa ciani ndi amphamvu ? Tingapewe bwanji kutengela anthu a makhalidwe oipa ? Komabe , pamene mukukulitsa luso pa udindo wanu , mosakaikila mungathandize kusintha zinthu zina mumpingo kuti uziyendela limodzi ndi gulu la Yehova . Malemba amaonetselatu kuti Mphukilayo ni Yesu Khristu . — Yes . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti sanali kufuna kukhala mfumu pa dziko lapansi ? 3 Anadzipeleka na Mtima Wonse — Ku Ghana Mfumu yakwela pa hachi yoyela , zimene zikuimila nkhondo yoyela ndiponso yolungama pamaso pa Yehova . Kupatsa kumalimbikitsa mgwilizano na ubwenzi ( Miyambo 27 : 11 ) Ndife otsimikiza kuti Yehova adzapitilizabe kuticitila zabwino ndi kutisamalila . Ndi zinthu ziti zimene zidzakhala zofunika kwambili m’dziko latsopano ? ( Amosi 3 : 3 ) N’cifukwa cake Malemba amatilimbikitsa kuti : “ Yandikilani Mulungu , ndipo iyenso adzakuyandikilani . ” — Yakobo 4 : 8 . 13 Khalanibe Auzimu Potumikila Mumpingo wa Cinenelo Cina Pa tsiku limene Yesu anakamba mawu amenewa , anamwalila na kuikidwa m’manda . Coyamba , anali kukonda Yehova ndi kuopa kumukhumudwitsa . Dokotala wina wochedwa Margaret Chan , mkulu wa Bungwe Loona za Umoyo pa Dziko Lonse , anati : “ Popeza kuti anthu ndi amene acititsa matenda obwela cifukwa cokoka fodya , maboma ndi anthu ndi amenenso angathetse vutoli . ” 118 : 22 . Komanso tikawaona , siticita zinthu monga kuti taona mngelo . Yehova afuna kuti atumiki ake azikondana ndi kutumikilana monga abale ndi alongo . 44,250,000 Mwina okalamba amenewa ndi acibale athu . Mwina mungaganize kuti ndi bwino kungosiya kutumikila Yehova kuti musakwiitse olamulila . 10 : 23 ) Kudziŵa mfundo imeneyi , kudzatithandiza kuvomeleza kuti Yehova ndiye wolamulila wathu . — Ŵelengani Miyambo 3 : 5 , 6 . Anthu ocilikiza mgwilizano wa zipembedzo amakamba kuti palibe cipembedzo cimene cingakhale ndi coonadi pacokha . NDI KUTI KUMENE NDIMAKAMBILANA NDI ANTHU ? ( b ) Kodi lemba lathu la caka ca 2014 ndi liti , ndipo n’cifukwa ciani ndi loyenela ? Tiyenela kuwayamikila amene atumikila zaka zambili . 46 : 11 ) Cacitatu , Yehova amakupatsani “ mphamvu yoposa yacibadwa ” kuti mukwanilitse utumiki wanu . Mavesiwa ndi amene Mboni za Yehova zimaŵelenga mu ulaliki . Mu 1980 , ofesi ya nthambi inatisankha kuti tikhale omasulila mabuku . Tinaona kuti sitinali oyenelela kugwila nchitoyo . Nanga ‘ tingamuone bwanji Mulungu ’ ? ( Miy . 1 : 1 - 4 ; Tito 1 : 7 - 9 ) Ndipo pamene tiŵelenga zofalitsa zathu , timayamba kuona zinthu mmene Yehova amazionela . M’nkhani ino , tidzakambilana mafunso aya : Kodi Yesu anacita bwanji na khalidwe la tsankho ? * Mwacitsanzo , Johannes Rauthe anapatsidwa nchito yokonza njanji . Yehova watipatsa ciyembekezo ca ciukililo . ( Mac . Iye anathetsa mavuto a Yosefe panthawi yoyenela ndiponso m’njila yoyenela . Kodi mungatsimikize bwanji kuti Baibulo ni “ mawu a Mulungu ” osati maganizo a anthu kapena nthano zabodza ? Anawathandiza ‘ kumvetsa ciliconse ’ cimene cinali cofunikila kuti am’kondweletse . Pemphelo lakhala ngati mankhwala amene nimamwa tsiku lililonse . Ciweluzo cimeneco cidzacitika cisautso cacikulu cikadzatsala pang’ono kutha . Atumiki a Yehova amafuna - funa nzelu yocokela kumwamba ndipo amakhala ogwilizana cifukwa ca cikondi ( Onani palagilafu 19 ) 24 : 45 ) Anthu a Mulungu lomba anali atamasukilatu kwa Babulo Wamkulu . Cifukwa cakuti mosiyana ndi alembi ndi Afalitsi amene anali ophunzila kwambili ndi kuziona kuti ndi anzelu , ophunzila a Yesu anali ofunitsitsa kuphunzitsidwa monga ana . Amalondawo anali kumuyang’anila pamene anali kuuza ngamila zao kulowela njila ya kum’mwela . Koma ngati wina walakwa , cimakhala capafupi kucita zinthu zoonetsa kukhumudwa . Paulo analemba kuti : “ Pakuti [ Kristu ] ayenela kulamulila monga mfumu kufikila Mulungu ataika adani onse pansi pa mapazi ake . Izi zimaphatikizapo zambili osati kudziŵa cabe dzina lathu . Timafunanso kuti azidziŵa kuti ndise anthu abwanji na kuti tacita zotani mu umoyo wathu . — Num . Mwacionekele , mukanacita monga mmene Aisiraeli anacitila . “ Kwa ine , kulemekeza mkazi wanga kumatanthauza kumuona kuti ni wofunika , ndipo sinifuna kucita ciliconse cimene cingam’khumudwitse , kapena kuwononga cikwati cathu . ” — Micah . Iye anati : “ Ndimadziŵa bwino kuti sindiyenela kuvala zovala zimene ndinali kuvala ndili wacinyamata . ” Zocitikazi zinanilikimbitsa kuti nizimuyamikila kwambili Yehova cifukwa ca thandizo lodalilika limene amapeleka kwa atumiki ake amene amaika zinthu za Ufumu patsogolo . Atate anali Msilamu ndipo amai anali Myuda . Anadziŵanso kuti watsala pang’ono kuphedwa mwankhanza . “ Atate anatumiza Mwana wake kuti akhale Mpulumutsi wa dziko . ” — 1 Yohane 4 : 14 . Tinamva kuti anthu ambili ku Bolivia anali kufunitsitsa kuphunzila Baibo , ndipo umoyo kumeneko unali wosalila zambili . 2 : 17 ) Kodi lamulo limeneli linali losafunikila kapena lopondeleza ? 5 : 2 - 4 ) Kukamba zoona , akulu amene amagonjela Mulungu na Khristu , mutu wa mpingo , amapindula komanso amapindulitsa nkhosa zimene akuziyang’anila . — Yes . Zimenezi zionetsa kuti mpingo ndi wamtengo wapatali kwa Yehova . Cinthu cimodzi cimene cingakuthandizeni kucita zimenezo ndi kuyamikila madalitso amene takhala tikulandila . Mmodzi wa io anafunsa mtsikanayo kuti , “ Kodi dzina la Mulungu ulidziŵa ? ” Conco , mu 1967 , tinakukila ku Adelaide m’dziko la Australia . Ngati tiuza Mulungu zakukhosi kwathu kupyolela mpemphelo , iye amayankha mapemphelo athu kupitila m’Baibulo , m’magazini athu , kapena pogwilitsila nchito Akristu anzathu . Zosankha zina zimakhala zazikulu kuposa zina . Ngati munayamba kale kucita zimenezi , ndiye kuti mukucita bwino . Ndithudi , Anna anatonthozedwa ndiponso anapeza cimwemwe cifukwa colambila Yehova . 17 : 3 ) Onse anali opanda ungwilo ndipo analakwitsa zinthu zina . Koma Asa sanacoke kwa Mulungu cifukwa mtima wake unali “ wathunthu ” kwa iye . Komabe , kuimba , kujambula zinthu , na kusangalala , sizinatsilize nkhawa zanga . 14 : 25 , 26 ) Kodi zimenezi zingatithandize bwanji monga aphunzitsi a uthenga wabwino ? Tinali kuona kuti utumiki umenewo udzakhala wokondweletsa . NYIMBO : 100 , 87 Koma sin’nalole ciliconse kunicititsa kuleka upainiya . ” Zimenezi zinakwiitsa Davide , cakuti anaganiza zokapha Nabala ndi anthu ake . Ponena za akulu mumpingo , Baibulo limatilangiza kuti tiyenela kutsanzila cikhulupililo cao . Tikasinkhasinkha ndi kupeza mayankho a mafunso amenewa tidzapindula kwambili poŵelenga Baibulo . Zimenezi zinasangalatsa mwini malowo kwambili cakuti analola banjalo kukhalabe pamalopo ndipo analionjezela malo olimapo . Mfundo zimenezi zilipo m’zitundu zosiyana - siyana pa webusaiti yathu . N’cifukwa cake panthawi ina , Rakele anakamba mokondwela kuti : “ Ndalimbana mwamphamvu . . . ndipo ndapambananso . ” — Gen . Iye anabatizika mosazengeleza . — Ŵelengani Machitidwe 22 : 12 - 16 . Iwo sanalole Mulungu kuwathandiza . Coonadi ca mtengo wapatali cokamba za Yehova , cinafika m’banja langa mu 1981 . Mkazi wanga Mairambubu , ndiye anali woyamba kumva coonadi . Mwacitsanzo , mwamuna wina wacikulile ndithu , dzina lake Jim , anati : “ Nthawi zambili ndinali kupempha Mulungu kuti andithandize kukhala wamtendele ndi wodziletsa koma pakangopita nthaŵi , mkwiyo wanga unali kubwelanso . Kodi mkazi angaonetse bwanji kuti amagonjela modzicepetsa ? ( b ) Kodi colinga cathu kweni - kweni poseŵenzetsa bwino ufulu wosankha zocita n’ciani ? N’cifukwa ciani tifunika kuyandikila Yehova ? Mau a Yehova anamveka kucokela kumwamba , kuonetsa kuti iye anali kucilikiza Yesu ndi kukondwela naye . ( Mat . Cifuno canga couzako ena za ciyembekezo ca kutsogolo cinakula . Conco , ine na amayi tinabatizika mu March 1940 mumzinda wa Dover . Ndiyeno ananiuza kuti anikonzela mphatso . Mphatso yake inali ndalama yokwanila kulipilila zonse zofunikila . ” PACIKUTO : Ofalitsa a Ufumu alalikila ku Santiago de Cuba , mzinda wina waukulu wa pa cilumba umene ndi wochuka cifukwa ca nyimbo za kumaloko ndi magule ake Eduardo anafunika kubweza nkhongole pang’onopang’ono , ndipo anafunikanso kupeleka ciongola dzanja pa ndalama zimene anakongola . Mungafunsile ku ofesi ya nthambi m’dziko limene mukhala kuti mudziŵe mmene mungacitile zimenezi . 5 , 6 . ( a ) Kodi munacita ciani kuti mukhale paubwenzi ndi Yehova ? Conco , khalani ndi colinga cokhala mmodzi wa anthu mamiliyoni ambili amene adzapezeka pa mwambo wa Mgonelo wa Ambuye , umene udzacitika pa Cisanu April 3 , 2015 dzuŵa litaloŵa . Kwa iye , “ magazi alionse ” ndi opatulika . Iwo atapita ku Russia kukaceza , anacita cidwi kuona anthu okondwelela amene anapezeka pa misonkhano koma panali abale ocepa cabe amene anali kucititsa misonkhanoyo . Kodi Mwavala Zonse za Nkhondo Yauzimu ? “ Ikani maganizo anu pa zinthu zakumwamba , osati pa zinthu zapadziko . ” — AKOL . Ganizilani mmene mudzamvelela mukadzapulumuka cisautso cacikulu monga mmodzi wa khamu lalikulu . Kodi inu mudzavomela mwa kutambasula dzanja lanu kwa Mulungu amene akulonjezani kuti : “ Usachite mantha . Kucoka kumanzele kupita kulamanja . Kumbuyo : Yaroslav , Pavel , Jr . , na Vitaly Pa 1 May , 1949 , n’nakhala mpainiya wa nthawi zonse . 8 : 20 ) Iye anadzipeleka kugwila nchito zotsika . Mukatelo mudzakhala otsimikiza kuti ‘ zinthu zidzakuyendelani bwino . ’ Natani anamuuza kuti : “ Citani ciliconse cimene cili mumtima mwanu , cifukwa Mulungu woona ali nanu . ” Uthenga wa Ufumu unakhaladi nkhani yosangalatsa kwambili mu 1914 . Conco , muzikhala chelu na kuona bwino - bwino mmene zinthu zilili mu umoyo wa munthu . Izo zimayesetsa “ kuvala umunthu watsopano umene unalengedwa mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu ndipo umatsatila zofunika pa cilungamo ceniceni ndi pa kukhulupilika . ” ( Ŵelengani Salimo 110 : 1 , 2 , 4 . ) Malangizo amene amapeleka kwa atumiki ake omvela a padziko lapansi , ndi othandiza kwambili ndipo ndi oyenela cakuti awathandiza ‘ kukonda malangizo . ’ Conco , ifenso tifunika kulemekeza ufulu wa ena pa zosankha zawo pa nkhani zaumwini . — 1 Akor . Nthawi zina , tingafunike kukambilana ndi munthu kangapo kuti tikhazikitse mtendele ( Onani ndime 15 ) Ciphunzitso ca Utatu : Patapita zaka pafupifupi 300 pambuyo pakuti Baibulo yatha kulembedwa , munthu wina wokhulupilila Utatu anawonjezela mawu ena pa 1 Yohane 5 : 7 akuti “ kumwamba , Atate , Mawu , ndi Mzimu Woyela : ndipo atatu amenewa ndi mmodzi . ” ( Ekisodo 18 : 21 , 22 ) Patapita zaka 40 , iye anatsindikanso kufunika kokhala ndi amuna anzelu , aluso ndi ozindikila kuti akhale oweluza anthu . — Deuteronomo 1 : 13 - 17 . Marita nayenso anali kukhulupilila kuti mlongo wake , Lazaro , “ adzauka pa kuuka kwa akufa m’tsiku lomaliza . ” — Yohane 11 : 24 . Ndi cikhulupililo cotani cimene tili naco mwa Yehova ? Komanso zimene mbalamezo zimacita zingakhale mafanizo abwino amene tingaseŵenzetse . Mwacitsanzo , lsaki , Yakobo , ndi Ahiya atakalamba , anafa maso . ( Gen . “ Ine na mkazi wanga tinali kuonetsa cidwi kwambili kwa ana athu , ” anatelo tate wina ku Japan wa ana aŵili . Iye anamva cisoni kwambili cakuti anafika pogwetsa misozi . — Yoh . 11 : 33 - 36 . Olo zili conco , niona kuti nifunika kupitilizabe kulimbana ndi vutoli . Citsanzo cawo cinanilimbikitsa kwambili . Emil Yantzen Ena angaganize kuti anchito amene anaseŵenza ola limodzi anafunika kulandila ndalama yocepa kuposa enawo . Koma mwini mundayo anaonetsa khalidwe la kukoma mtima kwakukulu kwa anchito amene anaseŵenza nthawi yocepa . Mulungu analenga angelo kuti azikhala kumwamba . ( b ) Kodi Paulo analangiza Timoteyo pa mbali zitatu ziti zokhudza kuphunzila ? Kodi nimayesetsa kuona ena mmene Yehova amawaonela ? ’ Yehova adzakondwela ngati tim’khulupilila ndi mtima wonse . ( Mateyu 26 : 52 ) Komabe , tifunika kutengela cikhulupililo ca Davide . Tingatengele bwanji citsanzo ca Yesu pankhani yokhala wolimba mtima ? Izi ziphatikizapo ciŵelengelo ca Mboni zonse zimene zikulalikila uthenga wabwino , kuculuka kwa zofalitsa zofotokoza uthenga wabwino , ndi kuculuka kwa zinenelo zimene tikugwilitsila nchito polalikila uthenga umenewu Tsopano dzuŵa linali litayamba kuloŵa . Habakuku akanakhala ndi maganizo amenewa , Yehova akanasiya kumukonda , ndipo mwacionekele akanaonongedwa panthawi imene Ababulo anaononga Yerusalemu . ( Sal . 37 : 28 ) Coyamba , afunika ‘ kufufuza na kufunsa ’ mafunso mosamala kuti atsimikizile ngati munthuyo anacitadi chimo . ▪ Yehova Ndi Mulungu Wacikondi Ndiponso , n’zosakayikitsa kuti Nowa anafotokozela anthu njila imene ingawapulumutse mwa kuwauza lamulo la Mulungu lakuti : “ Udzaloŵe m’cingalawaco . ” KHALANI WAUBWENZI : “ Wodzipatula amafunafuna zolakalaka zake zosonyeza kudzikonda . Iye amacita zosemphana ndi nzelu zonse zopindulitsa . ” ( Mat . 24 : 14 , 21 ) Motengela Nowa , tiyeni tikhale na cikhulupililo colimba , podziŵa kuti Mulungu adzagwapo lomba apa . Tikasankha kumumvela ndi kucita cifunilo cake , timaonetsa kuti timam’konda ndipo tifuna kum’kondweletsa . Zimenezi zamuthandiza kuti asamadzione ngati wosafunika . Akhristu afunika kutsatila mfundo za m’Baibo posankha njila ya cilezi . Conco , ngati mupanga zosankha zogwilizana ndi mfundo zimene Yesu anaphunzitsa , mudzapeza cimwemwe ndipo mudzakondweletsa Yehova . — Miy . Nikumbukila kuti usiku wina pa tsiku la mwambo wa Halloween , n’naona mwamuna wina ali pa khonde pa nyumba yake atavala malaya oyela na cisoti , monga mmene anthu a KKK anali kuvalila . Kafukufuku wina wa posacedwapa amene anacitika pakati pa anthu oposa 68,000 , anaonetsa kuti ngakhale nkhawa yaing’ono ingacititse munthu kufa msanga . Nanga tingaonetse bwanji kuti timawakondadi ? Kodi mwaona kuti ulosiwu ukugwilizana ndi ulosi umene taŵelenga pa Danieli 2 : 44 ? Komanso , cikondi “ cimakondwela ndi coonadi . Baibulo limakamba kuti sitiyenela kunyoza anthu . — Tito 3 : 1 , 2 . Ganizilani zopinga zimene mungakumane nazo ndi mmene mungazigonjetsele . Iye anali kusangalala kugwila nchito imeneyi cifukwa anali kudziŵa kuti ni anthu ambili amene anali kulandila cakudya ca kuuzimu . Anapempha mwamuna wake kuti apite ku msonkhano coyamba , pambuyo pake adzabwela ku cikondwelelo . Kwa zaka zitatu , iwo anali kunisonkhezela kuti niyambenso makhalidwe akale . ( Yobu 1 : 10 , 11 ) Ngakhale kuti mau a Satana anali kukhudza Yobu cabe , iye anatanthauzanso kuti anthu onse amatumikila Mulungu ndi mtima wadyela . Ni Yehova amene wacititsa kuti kupita patsogolo kumeneku kutheke . Baibo imakamba kuti uphungu wake ni wouzilidwa , komanso ni “ opindulitsa pa kuphunzitsa , kudzudzula , kuwongola zinthu . ” Mlongo wina dzina lake Shari amene ndi mpainiya anakamba kuti : “ Apainiya amaoneka olimba cifukwa nthawi zonse amakhala mu ulaliki . Mkristu wofikapo amayesetsa kuthetsa mikangano m’malo mokhala cokhumudwitsa kwa ena . Mzimayiyo sanafune kuti Yesu adziŵe . Koma Yesu anafunsa kuti : “ Ndani wandigwila ? ” Kodi Mfumu Davide anacita bwanji atauzidwa kuti mwana wake ndiye adzamanga kacisi wa Mulungu ? Poyamba zinali zovuta kuti iwo akambilane mwamtendele , koma zinthu zinasintha atayamba kukambilana nkhaniyo modekha . Amaona kuti Iye amapanga cabe malamulo ndi kulanga amene samumvela . M’caputa 4 anakamba za Abulahamu wokhulupilika . Kuganizila zimene zinacitikila Yehosafati kungamuthandize . Conco , pitilizani kukulitsa cikondi canu pa Yehova ndi kumukhulupilila kwambili . Nadia anati : “ Timakondwela na ŵanthu amene timakumana nawo mu ulaliki . ” Pambuyo pake , amandipatsa malangizo abwino koposa . ” Malinga ndi kopeyo ( Digest , 9.2.27.14 ) , katswili wa zamalamulo dzina lake Ulpian anakambapo za mlandu umene wolamulila waciroma Celsus anaweluza . Iwo sanali kulima ndipo anacita mantha kukhala m’midzi yopanda citetezo ndiponso sanali kuyenda pamseu kuopa kuti ana ao angatengedwe ndipo akazi ao angagwililidwe . ( 1 Sam . 1 : 4 - 7 , 10 , 16 ) Hana anakhutulila Mulungu nkhawa zake zonse na kum’lonjeza kuti : “ Inu Yehova wa makamu , mukaona nsautso yanga , ine kapolo wanu wamkazi , ndi kundikumbukila , ndiponso ngati simudzaiŵala kapolo wanu wamkazi ndi kum’patsa mwana wamwamuna , ndidzam’peleka kwa Yehova masiku onse a moyo wake , ndipo lezala silidzadutsa m’mutu mwake . ” * ( 1 Sam . Cifukwa cakuti Yesu anadziŵa zimene zinali pafupi kucitika . Mofananamo , ngati moleza mtima na mosalekeza makolo aphunzitsa ana awo ‘ malangizo a Yehova ndi kaganizidwe kake , ’ amawathandiza kukhala odzilanga okha ndi anzelu . — Aef . Mkhristu angasankhe kukhala na mfuti n’colinga cakuti aziphela nyama kuti azidya kapena kuti adziteteze ku nyama zolusa . Zilakolako zathu za ucimo zingakhale zamphamvu kwambili . M’dziko latsopano , tidzalandila mipukutu ya malangizo atsopano amene tidzayenela kutsatila ( Onani ndime 19 ndi 20 ) Komanso zingapangitse kuti zokamba za anthu onyoza zioneke monga zoona . Iwo amati : “ Kukhalapo kwake kolonjezedwa kuja kuli kuti ? N’takwanitsa zaka 18 , n’naganiza zocoka panyumba cifukwa ca nkhanza ya Atate . Nili nanzanga ku Sukulu ya Giliyadi Kodi Mbuye adzabwela liti kudzaŵelengela cuma cake ? Mwa kucita zimenezo , io anaonetsa zimene anthu a Mulungu anali kudzacita mtsogolo monga mmene mneneli Mika anakambila kuti : “ Mtundu uliwonse wa anthu udzayenda m’dzina la mulungu wake . M’kupita kwa nthawi , udzatsegula maganizo anu kuti mumvetsetse “ zinthu zozama za Mulungu . ” — 1 Akorinto 2 : 10 . 15 : 41 ) Nanga kodi iye amawaona bwanji anthu padziko lapansi ? Kale kukalibe intaneti , Mboni za Yehova zinali kudziŵika kaamba ka khama lao la kulalikila uthenga wabwino wonena za Ufumu wa Mulungu . Ndiponso , ziyeneletso za atumiki othandiza zipezeka pa 1 Timoteyo 3 : 8 - 10 , 12 , 13 . Timafunikila thandizo la Atate wathu wakumwamba , cifukwa sitingakwanitse kuwongolela mapazi athu . — Yer . Conco , tiyeni tipitilize kusinkhasinkha Malemba kuti timudziŵe bwino Yehova . Ananithandiza kuti nipezenso mphamvu mwauzimu ndi kuti nisafooke . ” Iwo ayenela kuti analamula anchito awo kuti aunyamule na kukauika m’manda . Apanso tinaona kuti Yehova anatithandiza mwacikondi . Iwo anali mbali ya ‘ mtambo waukulu wa mboni ’ zimene zinali ndi mwai wokhala mabwenzi a Mulungu . Yosefe anaona kuti kudzionetsela n’kosayenela cifukwa cakuti anali wodzicepetsa ndiponso anali ndi cikhulupililo . Atumiki a pa Beteli atsopanowa , amayamikila pamene abale anzao a pa Beteli ndi mumpingo wao akhala nao pa ubwenzi . Mose anapanga cosankha cabwino . — Ŵelengani Aheberi 11 : 24 - 27 . Iye anati : “ Pamene ndinaŵelenga magazini ndinadziŵa kuopsa kokoka fodya , ndipo ndinali kulimbikitsa anthu odwala kuti aleke kukoka . Kodi nkhani ya Abulahamu itiphunzitsa ciani zokhudza ciukililo ? ( Ŵelengani Yesaya 50 : 4 ; Aheb . Awa Ndi Malo Athu Olambilila Mafumu anayi aciyuda amene tinakambilana m’nkhani yapita , anatumikila Yehova ndi mtima wathunthu . [ 2 ] ( ndime 18 ) Pokambilana mfundo za m’Baibo zimene zingathandize banja lanu , ŵelengani nkhani yakuti “ Kulera Ana M’dziko Lachilendo — Mavuto ndi Mphoto Zake ” mu Nsanja ya Olonda ya October 15 , 2002 . N’zimene zinacitikila Joshua , amene tamuchula kuciyambi kwa nkhani ino . Kudzicepetsa kumatithandizanso kuvala mwaulemu , ndi kudzikonza mwacikatikati . Mlongo wina dzina lake Rhonna , amene amakhala ku Asia , anakamba kuti zimatenga nthawi kuti tione mmene Yehova amatithandizila pa umoyo wathu . Akulu kuphatikizapo ise tonse tiyenela kutengela citsanzo cake . — w18.04 , mape . Mau a Mulungu amachula imfa kuti ndi mdani ndipo akutilonjeza kuti “ idzaonongedwa . ” — 1 Akorinto 15 : 26 . Cimodzi mwa zinthu zimene zinali kum’detsa nkhawa kwambili , n’cakuti nthawi zina anali kulephela kuika maganizo ake pa zimene anali kuŵelenga m’Baibo na pa zinthu zina zauzimu . MFUMU ILINGANIZA NZIKA ZAKE KUTI ZIGWILE NCHITO YOCULUKA Sikuti Mulungu ndi wosamvetsetseka , iye amafuna kuti timudziŵe . — Machitidwe 17 : 27 . Komabe , m’zaka zaposocedwapa , tasiya kufotokoza pa zimene nkhani za m’Baibulo zimaimila . Yesu anali atacenjeza ophunzila ake kuti adzadedwa , adzazunzidwa , ndipo ena adzaphedwa kumene . Popemphela kwa Yehova , Yesu anati : “ Pakuti moyo wosatha adzaupeza akamaphunzila ndi kudziŵa za inu , Mulungu yekhayo amene ali woona , ndi za Yesu Khristu , amene inu munamutuma . ” ( Yoh . Izi zinacitika katatu konse . Tikatelo , tidzatha ‘ kutsatila mapazi ake mosamala kwambili ’ na ‘ kudzikonzekeletsa ndi maganizo ’ amenenso Khristu anali nawo . — 1 Pet . Mwacitsanzo , Yakobo anaonetsa cikhulupililo colimba m’malonjezo a Mulungu , ngakhale pamene anali wofooka , wosaona , ndiponso wodwala kwambili . ( Gen . Ndiyeno akazi aŵiliwa anayamba kulimbana kwambili ndipo nsanje imeneyo inayambukila ana onse pa nyumbapo . — Genesis 29 : 16 - 35 ; 30 : 1 , 8 , 19 , 20 ; 37 : 35 . Citsanzo cina ca m’Baibulo ni ca mtumwi Petulo . Monga wacinyamata , mungapange zosankha zimene zingakuthandizeni kuti mudzakhale ndi mipata ina yotumikila Mulungu mtsogolo . 7 , 8 . ( a ) Kodi akulu angatsanzile bwanji kaphunzitsidwe ka Yesu ? N’ciani cinacitika Manowa atapempha Yehova kuti amuthandize kukhala kholo labwino ? ( Machitidwe 16 : 25 ) Ndipo mzimu wa Mulungu udzakuthandizani kukumbukila zinthu zimene munaphunzila . Thomas anati : “ Maka - maka pa nkhani zofunika kwambili , ine na mkazi wanga timafuna kudziŵa ngati mwana wathu akumvetsetsa na kukhulupilila zimene tikumuphunzitsa . 7 : 7 ) Ndiponso , Mkristu aliyense ayenela kuvomeleza kuti mtima ndi wonyenga ndi kuti ungatitsutse ngakhale kuti Mulungu amakondwela ndi zocita zathu . ( Yer . 17 : 9 ; 1 Yoh . Conco , musamakhulupilile zilizonse kapena kuvomeleza zinthu m’cimbuli - mbuli . ( Yuda 14 , 15 ) Mwina mungadabwe kuti mu ulosi umenewu , Inoki anakamba monga kuti Mulungu anali atacita kale zimene ulosiwu unakamba . Iwo acokela m’mitundu yosiyanasiyana , m’maiko osiyanasiyana , ndipo aphunzila kukonda ndi kuopa Mulungu . Cifukwa ca makamela amenewa , munthu akaba amagwidwa mosavuta . 3 : 1 - 5 ) Ana sabadwa na nzelu zosiyanitsa cabwino na coipa . Iye analemba kuti : “ Tinali kukonda kwambili kuŵelenga kabuku kameneka ndipo kanali kutikumbutsa cithunzi ciliconse . ” 4 : 10 ) Ndipo pamene Yehova analonjeza za Mpulumutsi , kwa iye zinali monga kuti nsembeyo yapelekedwa kale . ( Afilipi 3 : 16 ) Mukamvela malangizo amenewo , mudzayamba kulakalaka kudzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa . Atagwila nchitoyo kwa zaka zambili , anapemphedwa kukagwila nchito m’khola la nkhuku pa famu yochedwa Kingdom Farm , ku New York . Nanga tingasankhe bwanji zinthu mwanzelu ? M’mbili yonse ya anthu mavuto akukulilakulilabe . Iye anadzudzula Davide mwaukali , ndipo anamunena kuti anabwela kukaonelela kuphedwa kwa anthu pa nkhondo . * N’nakambilananso ndi akulu ndiponso woyang’anila dela ndi mkazi wake za colinga canga cokatumikila ku dziko lina . Wacicepele amene amafunitsitsa kukondweletsa Yehova , amaona nchito yolalikila kukhala yofunika ngako . Ŵelengani 1 Mbiri 22 : 5 . Tilidi ndi mwai wolandila moyo wosatha . ( b ) N’ciani cimene tikuphunzila pa zitsanzo za anthu a m’Baibulo amene anaononga colowa cao cakuuzimu ? Tingacite ciani kuti tikailandile mphoto imeneyo ? Kodi Hava anali kuganiza kuti adzakhala ndi umoyo wotani ? ( Aroma 5 : 1 , 18 ; 8 : 1 ) Amenewa amachedwa ‘ odala ndi oyela , ’ ndipo ndi oyenelela ciukililo ca kumwamba . Mavutowa anayamba cifukwa Satana , Adamu , ndi Hava anapandukila Yehova . Tikutelo cifukwa cakuti mmene zinthu zilili masiku ano n’zofanana kwambili ndi mmene zinalili kwa Akristu a ku Yudeya . ( Maliko 14 : 53 , 54 , 66 - 72 ) Pambuyo pake , Petulo anamva cisoni kwambili ndi zimene anacitazo . Anthu amenewa angakhale ndi cidwi akayamba kumvetsetsa mmene dipo limene Yehova anapeleka limaonetsela cikondi ndi nzelu zake . Koma kuti tipitilizebe kukhala ndi moyo , timafunika cakudya . Ndithudi , zaka zambili - mbili m’mbuyomo , ulosi wa pa Salimo 118 : 22 unali utakambilatu za kuuka kwa Khristu kumene kunali kudzacitika zaka zambili m’tsogolo . Mwacitsanzo , ngati tifuna kupanga cosankha pankhani inayake , buku la Cingelezi lakuti Watch Tower Publications Index , ndi Buku Lofufuzila Nkhani la Mboni za Yehova , angatithandize kudziŵa maganizo a Yehova pankhaniyo . Ninamuyang’ana modabwa . Pamene ana athu aŵili , Gilly ndi Denise , anakwatiwa , tinatseka sukuluyo . Nayenso José wa zaka 73 , wa ku Brazil anati : “ Anthu amakondwela kukhala ndi munthu amene amawamvetsela , kuwaganizila , kuwayamikila komanso amene ndi wansangala . ” Pambuyo pake , Cecilie , anaganiza zofunsa Mboni za Yehova kuti apeze mayankho okhutilitsa pa mafunso ake . ( 1 Tim . 2 : 4 ) Conco , pamene uphunzila Mau a Mulungu na zofalitsa zathu , osangoŵelenga mwacisawawa yayi . N’zacisoni kuti Aisiraeli ena anakodwa m’zilako - lako zoipa cifukwa colephela kudalila Mulungu . Cina cimene cingatithandize kukhala pa ubwenzi wolimba na Yehova ndi kupewa kuloŵelela kwambili m’zamalonda m’dzikoli . M’malomwake , tifunika kufuna - funa cuma “ ceni - ceni ’ . Kodi Mumaona Kufunika Kopita Patsogolo Kuuzimu ? M’malo mwake , tizikumbukila kuti “ anthu osiyanasiyana ” angalandile uthenga wabwino . — 1 Akor . Komabe , ngati mwakonzekela pasadakhale , mumagwilizana m’banja , mumalankhulana bwino , ndipo koposa zonse ngati mumapemphela kwa Yehova , mudzakwanilitsa udindo wanu wolemekeza makolo anu okondedwa . Mabuku ena a m’Baibulo amafotokoza za mbili yakale , malamulo , ulosi , ndakatulo , miyambo , nyimbo , ndi makalata . Ayuda anzake anali kungomupitilila munthuyo , koma Msamariya anamumvela cifundo . Mwacitsanzo , ganizilani zimene zinacitika pamene Aisireli anazungulila Yeriko , mzinda wa Akanani . Ndiyeno mngelo anawongolela Sara mwa kufunsa kuti , “ Kodi pali cosatheka ndi Yehova ? ” Mmene mungacitile ndi nkhanza za kugonana ( Mac . 3 : 17 ; 17 : 30 ) Ngati tatsimikiza mtima kucita cifunilo ca Mulungu , Satana sangakwanitse kutitaitsa cikhulupililo cathu . — Yobu 2 : 3 ; 27 : 5 . Patapita zaka ziŵili , anayamba kuyenda na Paulo . Iye sanadziŵe n’komwe mmene tsogolo lake lidzakhalila . Ni lemba liti linam’thandiza ? Ngati n’conco , onani peji yothela ya magazini ino . Conco ngati mpainiya wafooka , tingamulimbikitse mwa kum’kumbutsa zabwino zimene wakhala akucita pothandiza ena . Pamene anali wamng’ono , iye anali kufuna kudzakhala pa nchito yapamwamba . Koma atayamba kugwila nchito yopanga ophunzila , anapeza cimwemwe ceni - ceni cifukwa anaona mmene anthu anali kusinthila miyoyo yawo atamva Mau a Mulungu . Mmene amakhalila umoyo wake zimaonetsa kuti ubwenzi wake ndi Yehova , ndiponso kukonda ena , ndi zofunika kwambili kwa iye . N’cifukwa ciani nchito ya Lefèvre d’Étaples inali yofunika kwambili ? Cinthu cinanso cimene ndi mbali ya cuma cathu cauzimu ni coonadi cimene tinaphunzila . Nanga tingaonetse bwanji kuti timacilikiza mokhulupilika gulu la Yehova ? 7 : 7 ; 1 Pet . Patangopita miyezi itatu , asilikali 30,000 aciroma akubwela mumzindawo motsogoleledwa ndi bwanamkubwa waciroma wa ku Siriya , dzina lake Seshasi Galasi . Tingaphunzile ciani pa citsanzo ca Hana ? Ngakhale kuti anthu anali kuwalandila ndi kuwaceleza , Yesu ndi atumwi ake anali kunyamula “ bokosi la ndalama . ” Izi zionetsa kuti io sanali kungodalila thandizo la anthu . ( Yoh . Anali kugwilitsila nchito mau ogwila mtima ndi osavuta kumva . Mu 1973 , ndinabatizidwa . Koma ambili aona kuti kukambitsilana kwa conco kwakhala kothandiza . Mfundo imeneyi imagwilanso nchito kwa Mkhristu amene apitiliza kugwila nchito imene imafuna kuti azinyamula mfuti . 6 : 6 , 7 ) Ndipo muziyesetsa kucitila nao zinthu pamodzi . N’ciani cingatithandize kukhalabe okhulupilika kwa Yehova ? Iwo sanafunike kutengela anthu olambila milungu yonama amene anali kukhala nawo pafupi . Mpingo wa kumeneko unapeleka ndalama na katundu wa m’nyumba . KODI KUKHULULUKA KUMATANTHAUZA CIANI ? Ngakhale Yesu anakamba kuti Mulungu “ amadziŵa zimene mukufuna musanapemphe n’komwe . ” Koma m’kupita kwa nthawi , anthu angaleke kukuonani kuti ndinu “ mlendo . ” Kodi kudziŵa kuti Yehova ndi mfumu yamuyaya kuyenela kutipangitsa kucita ciani ? 73 : 28 ; Yak . “ Mariya . . . [ anali kumvetsela mau a Yesu ] . . . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana makhalidwe ena aŵili a Yesu ocititsa cidwi , omwe ndi kulimba mtima ndi kuzindikila . Yehova anali kuona Aisiraeli monga anthu ake , ngakhale asanawakhazikitse kukhala mtundu . Kuyambila nthawi imeneyo , lamulo limeneli likali kugwila nchito m’Chechi ca Roma Katolika . Poika lamulo limeneli , chechi cinateteza udindo na cuma , zimene zinawonongeka pamene abusa amene anali pabanja analemba wilo kuti ana awo adzatenge katundu wa chechi . Pamene Adamu anasankha mwadala kusamvela Mulungu , anacimwa ndipo zotulukapo zake n’zakuti anataya moyo wangwilo — moyo wa Adamu . Koma io sanatsatile citsanzo ca atate ao ndipo anakhala anthu oipa . Marita anati : “ Ambuye , kodi sizikukukhudzani kuti m’bale wangayu wandilekelela ndekha nchito ? Mkazi wina amene wakhala m’cikwati kwa zaka 22 , amene cikwati cawo cinatsala pang’ono kutha , anakamba kuti : “ Tonse ndise obatizika , koma tinakhumudwitsana kwambili ndipo sitinali kugwilizana . Mike anati : “ Ndimapeleka citsanzo cabwino mwa kutsatila malangizo a gulu la Yehova . Zotulukapo zake n’zakuti , mu 2017 , anthu amene anapezeka pa Cikumbutso m’matauni atatu amenewa anali ambili kuŵilikiza kaŵili ciŵelengelo ca ofalitsa , kapena kuti hafu ya anthu onse a m’matauniwa . Tiziwaganizila acibululu osakhulupilila . Kodi Ndani Amadziŵadi Zamtsogolo ? 23 : 22 ; Aef . 6 : 1 - 4 ) Komabe , nthawi zina makolo atsopano m’coonadi angafunike thandizo la ena ndipo amaliyamikila kwambili . Yehova amadziŵa bwino mavuto amene timakumana nawo mu ulaliki . Taona kuti Yehova akutsogolela atumiki ake masiku ano otsiliza . Ndinaganiza zosiya kuyenda pa njinga yanga ya moto ndikuyamba kuyenda pabwato . Cifukwa cakuti siinali nthawi yoti afotokoze zinthu zonse zodabwitsa zimene anaona m’masomphenya ake . N’ciani cingacitike ngati cikumbumtima cathu n’cosaphunzitsidwa bwino ? Masiku ano , anthu a Yehova sakumana ndi ampatuko mumpingo . ( Machitidwe 4 : 24 , 30 ) Conco , ophunzila a Yesu anatsatila malangizo ake pankhani ya pemphelo . Simungadziŵe mmene lemba loyenelela lingakhudzile anthu . Kodi mwina Eliya sanali kufuna kupatsako ena mwai ndi nchito zina zimene anali nazo ? Pa cifukwa cimeneci , atumiki a Mulungu anali kulankhula ndi anthu osiyanasiyana , kuphatikizapo Ayuda amene anali mu Ufumu wonse wa Roma ndipo izi zinathandiza kuti uthenga wabwino ufalikile . Onani kuti Yesu anauza atumwi ake kuti : “ Atate amalemekezeka mukapitiliza kubala zipatso zambili ndi kusonyeza kuti mulidi ophunzila anga . ” Iwo sadzalandila mphoto yao ya kumwamba . ( Ŵelengani Salimo 37 : 10 . ) Posacedwapa , tonse , kaya ndife acinyamata kapena acikulile , tidzafunika kwambili thandizo la Akristu anzathu . ( Sal . 45 : 4 ) Yesu adzacita “ zinthu zocititsa mantha ” kwa adani ake pamene adzakwela pa hachi yake ndi kuononga dziko la Satana pa Armagedo . Mofanana ndi Abele na Inoki , iye anali kukhulupilila kuti “ mbewu ” yochulidwa mu Edeni idzaphwanya mutu wa njoka . — Gen . Iye anali kuonedwa kukhala mnyamata wapadela kwambili ku Babulo . “ [ Mboni za Yehova ] zili ndi makhalidwe abwino kwambili . Koma msonkhano utatha , io anayamba kutimenya . Kodi tiyenela kuimba mlandu Mulungu cifukwa ca mavuto athu ? Iye anaonetsa kuti amakonda kwambili Mulungu na anthu mwa kupeleka moyo wake monga nsembe . ( Akolose 1 : 3 ) Paulo analembelanso okhulupilila anzake kuti , ‘ m’dzina la Ambuye wathu Yesu Kristu , nthawi zonse muziyamika Mulungu , Atate wathu , pa zinthu zonse . ’ 71 : 15 , 16 . MAI wina dzina lake Anita , * atabatizidwa kukhala wa Mboni za Yehova , mwamuna wake anayamba kumutsutsa koopsa . ( Mat . 24 : 31 ) Odzozedwa amene ‘ adzatengedwa ’ ‘ sadzagona mu imfa , ’ m’lingalilo lakuti sadzakhala akufa kwa nthawi itali . Paulo polembela okhulupilila anzake , anachula njila imodzi imene tingaonetsele makhalidwe amenewa . Iye anati : “ Pitilizani kulolelana ndi kukhululukilana ndi mtima wonse , ngati wina ali ndi cifukwa codandaulila za mnzake . ( 1 Samueli 1 : 11 ) Mnazili anali kuloledwa kukwatila komanso kukhala ndi ana . Komabe , ana ena amene anasamukila m’dziko lina akaphunzila cikhalidwe na citundu ca m’dzikolo , amalephela kukamba citundu ca makolo awo kapena safuna kucikamba . Pamene Paulo anayamikila Akorinto cifukwa cogwilitsila nchito uphungu umene anawapatsa , analimbikitsidwa kupitiliza kucita zabwino . ( 2 Akor . Olo kuti Wycliffe anali atafa kale , iwo anamuweluzabe kuti anali wampatuko . Ngakhale kuti mlimi amagwila nchito mwakhama ndi kubyala mbeu , iye sangafulumizitse nyengo kapena kulamulila mbeu kuti zikule msanga . ( Dan . 12 : 3 ) Anzao okhulupilika a Akristu odzozedwa amenewa ayeletsa miyoyo yao ndipo ndi anamwali mwakuuzimu . Iye ‘ anaona cipulumutso ca Yehova , ’ ndipo anadziŵa kuti Yehova adzamenyela nkhondo Aisiraeli . Ndipo dziŵani kuti panthawiyo ndife cabe amene tidzakhala tikutsatila citsanzo ca mneneli Danieli mwa kupitilizabe kulambila Mulungu zivute zitani . — Dan . Munthu mmodzi amene sanachulidwe m’nkhaniyo anali Tatenai . Pambuyo pake anaphunzila za Yehova ndipo anafuna kukhala bwenzi lake . Mwacikondi , Yehova amafuna kuti mukhale ndi mwai womutumikila ndi kuonjezela utumiki wanu . Ndiyeno , Paulo anakamba mau oonetsa kuti palinso ena amene adzaukitsidwa kuti akakhale kumwamba . Iye anati : “ Aliyense pamalo pake : Coyamba Khristu , amene ndi cipatso coyambilila , kenako ake a Khristu pa nthawi ya kukhalapo kwake . ” — 1 Akor . Anthu ena amaganiza kuti kukhala na ufulu woculuka n’kumene kungawathandize kukhala na umoyo wabwino . Conco , ine na mwamuna wanga tikafuna kupita kukawaona , tinali kupemphela kwa Yehova kuti akatithandize kuyankha modekha ngati atikambitsa mwaukali . Lomba tiyeni tikambilane mbali zinayi izi zokhudza cilango : ( 1 ) kudzilanga wekha , ( 2 ) cilango ca makolo , ( 3 ) cilango ca mu mpingo , ndi ( 4 ) cinacake coŵaŵa kuposa ululu wa cilango . Conco khalani maso , pakuti simukudziŵa nthawi yobwela mwininyumba . Simukudziŵa ngati adzabwele madzulo , pakati pa usiku , atambala akulila , kapena m’maŵa , kuti akadzafika mwadzidzidzi , asadzakupezeni mukugona . Iye anati “ Nimakonda kuphunzitsa anthu za Yehova . Koma sin’naganizilepo kuti ningakwanitse kukatumikila kudziko lina . ( 1 Yohane 4 : 8 ) Ndiye cifukwa cake Yesu atafunsidwa kuti lamulo lalikulu pa malamulo onse ni liti , iye anayankha kuti : “ Uzikonda Yehova Mulungu wako ndi mtima wako wonse , moyo wako wonse , ndi maganizo ako onse . ” Ndipo vesi yoyamba m’caputa imeneyo imakamba za “ amene ali ogwilizana ndi Khiristu Yesu . ” Kodi iye anakopeka na umoyo wabwino , mwina wapamwamba kuposa umene anali nawo ku Uri ? 6 : 24 ) M’kupita kwa nthawi , kukonda kwawo Cuma kumatsiliza cikondi cimene anali naco pa Mulungu . — Mat . N’cifukwa cake Paulo analemba kuti : “ Musamade nkhawa ndi kanthu kalikonse , koma pa ciliconse , mwa pemphelo ndi pembedzelo , pamodzi ndi ciyamiko , zopempha zanu zidziŵike kwa Mulungu . 20 : 15 . Yosimbidwa ndi Corwin Robison Mfumu Davide analemba kuti : “ Wodala ndi munthu amene amacita zinthu moganizila munthu wonyozeka . Posapita nthawi , pamene tinali kutumikila monga apainiya a nthawi zonse , Atsushi anaikidwa kukhala woyang’anila dela wogwilizila . Ngati sacitapo kanthu , cikhulupililo cake cimakhala copanda phindu . Nanga tiyenela kuganizila ciani posankha cithandizo ca mankhwala ? Nthawi zambili , odwalawo amapezeka na matenda ena aakulu amene amawapangitsa kulephela kudzisamalila okha . Pofika m’nthawi ya Inoki , amene anali ambuye awo a atate ake a Nowa , anthu anali kucita zinthu zoipa kwambili . Ndi malangizo otani amene Paulo anawapatsa ? Zoona , timagwila nchito pamodzi na Mlengi , amene amaona kukoma mtima kumeneko monga nkhongole imene tamukongoza . Ganizilani cabe za cisoni , kulila , na kuvutika , kaamba ka anthu ambili - mbili amene anafa . Nkhani ino idzayankha mafunso aŵili oyamba . N’cifukwa ciani tingati galeta la Yehova lili pa liŵilo ? ( Ŵelengani Mateyu 6 : 19 - 21 . ) Yesu anakamba kuti mukadzaona “ zinthu zonsezi ” mukadziŵe kuti mapeto ali pafupi . Gary Breaux Tikadziŵa mmene kuika abale pa udindo kumacitikila , tidzamvetsetsa mmene mzimu woyela umagwilila nchito pankhani imeneyi . Ngakhale kaganizidwe kathu n’kocepa kwambili poyelekeza ndi ka Mulungu . Koma munthu amene amatha kuseŵenzetsa bwino cidziwitso ndi kumvetsa zinthu , ndiye timati ali ndi nzelu . — w16.10 , peji 18 . Kodi mumaganizila zokwatilana na munthu wina ? N’cifukwa ciani tifunika kukambilana mmene tingatonthozele ofedwa ? Motelo , Cisautso cacikulu cisanayambe , odzozedwa onse okhulupilika amene adzakhala akali padziko lapansi adzalandila cidindo cao cotsiliza . Kuti zikwanitse kugwila nchito yophunzitsa imeneyi , Mboni za Yehova zimasindikiza Mabaibulo pafupifupi 1.5 biliyoni , mabuku , magazini , ndi zofalitsa zina zothandiza pophunzila Baibulo caka ciliconse m’zinenelo 700 . 28 Mbili Yanga ​ — N’nasiya Zinthu Zina Pofuna Kutsatila Ambuye 103 : 9 ) Cotelo , tisaziganiza kuti Mulungu sangadalilenso munthu amene anacitapo chimo lalikulu . Iye ayenela kuti anali wacicepele pamene anatengedwa kwa makolo ake kupita ku Babulo . Asayansi ena akuona kuti n’zovuta kudziŵilatu zotulukapo zimene zingakhalepo cifukwa ca kuonongedwa kwa dziko . A Daka : Ndikuganiza kuti anthu amakamba conco cifukwa cakuti mumadzicha kuti Mboni za Yehova osati Mboni za Yesu . Titafika ku Florida mu November 1962 , tinadabwa pamene tinamva kuti kumeneko abale aciyela na acikuda sanali kufuna kusonkhana pamodzi kapena kulalikila m’dela limodzi . Komabe , ngati agwilitsila nchito zimene waphunzila , ndi kuseŵenzetsa cidziŵitso na kumvetsa zinthu m’njila yoyenela , ndiye kuti wayamba kukhala wanzelu . Khalani ndi Banja Lolimba ndi Lacimwemwe Baibulo limatitsimikizila kuti Mulungu adzacitadi zimenezi mtsogolo . Zimenezi zingacitike ngakhale titacita zilizonse zimene tingathe . Cotsiliza , yesetsani kuganizila za munthuyo . Pambuyo pakuti zakhala pa dzuŵa masiku atatu kapena asanu io anali kuzitembenuza n’kuzisiyanso padzuŵa masiku ofananao . Komabe , cimwemwe cimene tinali naco cinali cacikulu kuposa mavuto amene tinali kukumana nao . ( b ) Ni mavuto ati amene Akhristu onse amakumana nawo ? ( 2 Ates . 1 : 6 - 10 ) Panthawi imeneyo , iye sadzamvelanso cifundo anthu amene adzawaweluza kuti ni oipa . Iye anacita zimenezi ngakhale kuti alonda anali pomwepo . — Mac . 5 : 18 - 23 . Monga taonela , angelo abwino amagwilitsila nchito moyenela mphamvu zao . Ngati wodwalayo akukwanitsa kukamba ndipo angakonde kukambapo maganizo ake , cingakhale bwino kumufunsa kuti asankhe munthu amene angazim’pangila zosankha zikafika poti iye sakwanitsa kukamba . ( Miy 1 : 5 ) Funsilani ku maofesi a boma amene amapeleka thandizo kwa okalamba kuti mudziŵe thandizo limene makolo anu angalandile . Malinga ndi zimene tafotokoza , kodi tinganenenji ? Nowa anayenda ndi Mulungu mofanana ndi Inoki , ambuye wawo wa atate ŵake . Kodi Yesu anacita msonkhano wanji ndi ophunzila ake patsiku limene anaukitsidwa ? Ndipo anawathandiza kumvetsetsa udindo wao uti ? Motelo , abale pafupifupi 5,000 anagwilizananso ndi gulu . Koma panthawiyo , Mose anali kufuna kudziŵa ngati Mulungu anali wokonzeka kumuthandiza . Ndipo mau otsatilawa akukwanilitsidwa . Mauwo amati : “ Cilengedwe conse cikubuula limodzi ndi kumva zowawa mpaka pano . ” ( Eks . 12 : 48 , 49 ) Conco , Yehova anawalola kukhala nzika za mzinda wa anthu ake osankhidwa . — Num . Mwacitsanzo , mlongo Tiffany wa ku Australia , amene ni mpainiya , anaphunzila Ciswahili n’colinga cakuti azithandiza mpingo wa Ciswahili mumzinda wa Brisbane . Komabe , mwina mumadzifunsa kuti : ‘ Kodi Mboni za Yehova ndani makamaka ? Ngakhale kuti anthu ayesa - yesa kuthetsa njala , wokwela pa hosi yakuda akupitiliza kuthamanga . Zocita zathu zidzathandiza anthu ena kuzindikila kuti ndise anzelu ndi oganiza bwino . Kuphunzila zimene Baibulo limanena zokhudza Ufumu wa Mulungu ndi kosangalatsa . — Ŵelengani Luka 18 : 16 , 17 ; Yohane 4 : 23 . 17 , 18 . ( a ) Ndi mfundo zothandiza ziti zimene taphunzila m’mafanizo atatu amene takambilana ? Muzim’tumikila , kum’mamatila . ” — DEUT . Kumagwilizanitsa anthu osiyana mitundu , kocokela , ndi zinenelo kuti azitumikila Yehova mwacimwemwe ndi “ mogwilizana . ” ( Zef . Pokambilana funso lililonse , ganizilani zimene mungacite potengela citsanzo ca Atate wathu wakumwamba . — Ŵelengani Aefeso 5 : 1 . 8 : 30 . ( b ) Ni malangizo ati amene Yesu anapeleka kwa otsatila ake ? ( Mateyu 5 : 3 ) Conco , njila yabwino yokhutilitsila zosoŵa zimenezo ndi kukambilana ndi Mulungu nthawi zonse . Komabe , zimene Baibo imaphunzitsa ni nkhani yofunika kwambili kwa inu . Koma cosapeweka n’cakuti , kuyambila kwa Adamu , m’badwo uliwonse umakalamba ndi kuloŵedwa m’malo ndi wina . ( Mlal . Iye anasintha umoyo wake ndipo anakhala wofatsa ndi wodzicepetsa , conco ndinakondwela naye kwambili . N’ciani cimene tingacite ngati kulema na kutangwanika kumatilepheletsa kuceleza ena kapena kukaceza kwa Akhristu anzathu ? Koma Yehova anaona zinthu mosiyana ndi Gidiyoni . N’zimene Yesu anacita kwa ophunzila ake . Iye adziŵa kuti watsala ndi kanthawi kocepa . Conco amayesabe kutiletsa kulambila Yehova . — Chivumbulutso 12 : 12 . Zimenezi zinacitika pa May 22 m’caka ca 2000 . Popeza mizinda yothaŵilako inalipo , munthu amene wapha mnzake mwangozi sanali kuthaŵila kudziko lina , kumene akanayamba kulambila mafano . Mwacitsanzo , pa Agalatiya 4 : 21 - 31 , mtumwi Paulo anafotokoza za “ tanthauzo lophiphilitsila ” lokhuza akazi aŵili . Komanso Maxim anabatizika ali na zaka 11 , ndipo mlongosi wake Noemi anabatizika ali na zaka 10 . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Valani . . . kuleza mtima . ” — Akolose 3 : 12 . Nanga n’cifukwa ciani zili conco ? Coyamba , tiyenela kudzifunsa kuti , ‘ Ngati ine ndinali munthu winayu , kodi ndingafune kuti iye andicitile ciani ? 37 : 5 . Pambuyo pakuti cipupa ca Berlin cagwetsedwa , Mboni za Yehova zinapatsidwa ufulu wolambila . Ndiye cifukwa cake anaona kuti wacikondi wake anali “ monga mtengo wa maapozi pakati pa mitengo ya m’nkhalango , . . . pakati pa ana aamuna . ” — Nyimbo 2 : 3 , 9 ; 5 : 14 , 15 . Rutherford , pulezidenti wa Watch Tower Society panthawiyo . Iye anacita zoyenela ndipo “ anafunafuna Yehova ndi mtima wake wonse . ” ( Mat . 18 : 8 , 9 ) Mwacitsanzo , ngati anzanu ena amakutunthani kucita zinthu zokhumudwitsa Yehova , muyenela kuleka kugwilizana nawo . Apainiya atsopano anawonjezeka ku Britain Ndiyeno anapeleka malangizo awa : “ Conco tulukani pakati pao , lekanani nao . ” — 2 Akorinto 6 : 14 , 15 , 17 . 13 : 34 , 35 ) Pa mfundo imeneyi , Malemba amatilimbikitsa kuti tiyenela kukhala na “ maganizo ” amenenso Yesu anali nawo . Mwacionekele , Ahabu sanaphe Beni - hadadi cifukwa cofuna ndalama . Nkhani imeneyi ikufotokoza cifukwa cake kugwila nchito ndi Mulungu kumatibweletsela cimwemwe cacikulu . Conco , muziphunzila ndi ana anu buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa , ndiponso la “ Cikondi ca Mulungu , ” ngakhale kuti mwamuna kapena mkazi wanu satumikila Yehova . Ataona kuti zakudyazo sizinagwile nchito , abale ndi alongo ambili anakhumudwa . Corinna anali wosangalala kwambili ndipo sanaone kuti analakwitsa kupanga ulendo wautali umenewo . Ponena za Yesu mutu wa mpingo , Baibo inakambilatu kuti : “ Sadzaweluza potengela zimene wangoona ndi maso ake , kapena kudzudzula potengela zimene wangomva ndi makutu ake . Zimene zacitika m’mbili ya anthu zidzakhala umboni wakuti anthu opanduka ayenela kuonongedwa mwamsanga . M’buku la Danieli , timaŵelenga za acicepele anai aciheberi awa ; Danieli , Hananiya , Misayeli ndi Azariya . Pamene n’naphunzila zambili za m’Baibulo , n’naona kuti nifunika kusintha khalidwe langa . Kodi zimenezo zingasonyeze kuti ndinu munthu wokayikakayika ? Nanga kusinthako n’koyenela ? M’ceni - ceni anali kutanthauza Ophunzila Baibo . ( Deut . 30 : 16 ; Aheb . 13 : 7 , 17 ) Mzimu wosuliza kapena kukana malangizo ulibe malo m’gulu la Mulungu . Ngakhale n’conco , tingathe kulidziŵa bwino khalidwe la kudziletsa ndi kutengela citsanzo ca Yehova mwa kupenda mmene iye waonetsela khalidweli . Anthu amenewo anali kumuzonda ngako . 4 , 5 . ( a ) Kodi Aisiraeli anacita ciani kuti mizinda yothaŵilako isakhale yovuta kufikako ? Koma zambilinso zimakhala zabodza , zacabecabe , ndi zoipa . Adani anu akucita phokoso . Anthu odana nanu kwambili atukula mitu yao . Mwacitsanzo , mwana angadziyelekezele kuti wakwela pa gulugufe . Koma ena amaona zinthu mosiyanako . Delphine anapeza thandizo m’Baibo pa nthawi yovuta imeneyi . 105 : 19 ) Pamene mayeselo amenewo anatha , Yosefe anayenelela kulandila udindo wapadela . Kodi linawalanda ufulu anthuwo ? Mfundo yake ni yakuti , ngakhale kuti iwo anaiŵala mmene Yehova anawapulumutsila , iye sanawaiŵale anthu akewo . Anthu ambili amakhala ndi nkhawa komanso mantha akaganizila nkhaniyi . Mwacitsanzo , Mulungu anapatsa Adamu ulamulilo pa zamoyo zonse ndiponso nchito yaikulu koma yosangalatsa yakuti ache maina zinyama zonse . ( Gen . Mmene ‘ Tingayankhile Munthu Wina Aliyense ’ , 5 / 1 5 : 28 , 29 ) Conco , Mkhristu afunika kupewa kutamba zamalisece kapena kumvetsela nyimbo zolimbikitsa ciwelewele . Iye anati : “ Anzanga a mumpingo ananithandiza m’njila zambili ! ( Machitidwe 2 : 6 - 12 ) Koma zocitika zodabwitsa zotele sizicitikila Mkristu aliyense amene wadzozedwa . 2 : 2 , 3 ) Tili na Sukulu ya Apainiya , Sukulu ya Alengezi a Ufumu , Sukulu ya Giliyadi , Sukulu ya Atumiki Atsopano a pa Beteli , Sukulu ya Oyang’anila Madela ndi akazi awo , Sukulu ya Akulu , Sukulu ya Utumiki wa Ufumu , na Sukulu ya ziwalo za Makomiti a Nthambi ndi akazi awo . Mlongo amene anali kuphunzila naye , anapemphela kwa Yehova ndipo anaganiza zoleka kuphunzila naye . Ndine wokondwela ngako kuti n’nasankha kucita zambili pa nchito yopanga ophunzila . ” — Mlal . Mwacitsanzo , pewani kupezeka m’zocitika zimene zingakuikeni pa ciyeso . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Zolinga za munthu wakhama zimam’pindulila . ” — Miyambo 21 : 5 . Inde , tiyeni tiziimba mosangalala ! — Sal . Mlongoyu anakamba kuti : “ Zinali ngati kuti Yehova akukamba ndi ine usikuwo . Conco , m’pomveka kuti Davide analangiza Solomo kukhala wolimba mtima kuti amange kacisi . Boazi anabala Obedi , amenenso anadzabala Jese . — Rute 4 : 17 , 20 - 22 ; 1 Mbiri 2 : 10 - 12 . 19 , 20 . ( a ) Kodi zimene takambilana zigwilizana bwanji na mau amene Marita anakamba kwa Yesu ? Umenewu ndi umboni wakuti ali ndi cikondi cosatha kwa ife . Kukonda Mulungu ndi mtima wathu wonse , moyo wathu wonse , ndi maganizo athu onse kudzatithandiza kuphunzila Mau ake mwakhama . Ganizilani mmene munacitila pamene cikhulupililo canu cinayesedwa . Ngakhale n’telo , Yesu anaphunzitsa otsatila ake kuyembekezela Ufumu wa Mulungu . Koma tinaona kuti Arthur anayenela kupita ndithu kusukulu olo kuti zimenezo zikanacititsa kuti ine nikhale nekha . Koma musaiŵale kuti : Kukhulupilila Mulungu ndiye kungakuthandizeni kusaopa anthu . 7 , 8 . ( a ) Kodi makhalidwe a anthu anaipa motani m’nthawi ya Nowa ? ( Ŵelengani Aefeso 5 : 1 , 2 . ) M’maiko osauka , anthu ambili amafuna cabe kukhala ndi ndalama kuti agule foni , honda , kapena malo ocepa okhalapo . Apa tingakambe kuti Yehova anali kuuza anthu ake kuti , “ Ngati mudzakhalabe ku mbali yanga , na ine nidzakhalabe ku mbali yanu . ” Nanga n’ciani cingathandize atumiki a Yehova kukhala opanda nkhawa pamene akukalamba ? Yehova ni Mulungu wokoma mtima kwambili , ndipo amaona zabwino mwa ife monga mmene anacitila ndi mafumu anayi amene takambilana . Iye sanayembekezele Yaeli kucita zinthu zosiyana ndi zimene mwamuna wake akanacita . Coyamba , tiyenela kuzindikila kuti sindife amene tingapangitse kuti wophunzila Baibulo apite patsogolo kuuzimu . Yesu sanali kufuna kupeza anthu amene adzam’cilikiza ndi kumuteteza kwa adani ake . Koma zioneka kuti sanalimbe mtima kuti asinthe . Iye ndi Joe , mlongosi wake wamkulu , anathamangitsidwa panyumba ndi makolo awo okangalika a chechi ca Orthodox cifukwa cokana kuleka kuphunzila Baibo . Ndipo anaikamo zonse zofunikila kuti tisangalale na moyo kwamuyaya . — Genesis 2 : 8 , 9 . Masiku ano , zofalitsa zathu zimapezeka m’zinenelo zoposa 700 , ngakhale kuti zina mwa zinenelozo zilibe zofalitsa zina . Nkhaniyi idzafotokoza mmene ise tingapezele citonthozo , ndiponso mmene tingatonthozele ena amene afedwa . ( Aef . 4 : 24 ) Amene amavala umunthu watsopano amacititsa ziwalo za thupi lao kukhala “ zakufa ku dama , zinthu zodetsa , cilakolako ca kugonana , cikhumbo coipa , ndi kusilila kwa nsanje . ” M’baleyo anadalila Yehova kwambili . Conco , ulosiwo unali cenjezo kwa anthu onse . Unaonetsa kuti khalidwe lawo linafika poipa kwambili kucokela pamene anthu oyambilila anacotsedwa m’munda wa Edeni . Kodi n’kulakwa kufunsa moona mtima mafunso okhudza Baibulo ? “ Tinali kuseŵenzetsa ma baketi powasha m’malo mwa mashini yowashila , ” anatelo Adria . Ndiyeno , pakutsatila hosi yacitatu yakuda bii . Wokwelapo wake wanyamula sikelo pamene uthenga wacisoni wokamba za kucepa kwa cakudya ukulengezedwa . Kuonjezela apo , onetsetsani kuti mukuyamikila wophunzilayo cifukwa ca khama lake poyesetsa kutsatila zimene munamuuza kucita . Conco , nthawi zina muzipatula nthawi yoitana anzanu . Ndipo adzakuthandizaninso kuonetsa cikondi kwa ana anu , kukhala odzicepetsa , ndiponso ozindikila . Akulu sacita zinthu mozizwitsa . Kumanzele : Nadia na Marie - Madeleine . Inde anatelo , koma osati mwa mphamvu zao . ( b ) Ni mfundo iti imene tiyenela kukumbukila ngati takopeka ndi anthu oipa ? ( Yes . 48 : 17 , 18 ) Kugwila nchito yolalikila kumalemekeza Yehova komanso kumaonetsa kuti timamvela cifundo anthu . Yesu anakamba kuti Yehova “ adzapeleka moolowa manja mzimu woyela kwa amene akum’pempha . ” — Luka 11 : 13 . “ Khalani maso . Mauthenga Abwino safotokoza zonse zimene Yesu anakambilana na Mateyu . Komabe , iye anavomela ciitano ca Yesu cakuti akhale wotsatila wake . Apa Paulo anali kukamba zimene Yehova amacita pamene tikumana ndi mayeselo , osati tikalibe tikukumana nawo . N’ciani cinalimbikitsa banjali kupitiliza kutumikila m’dzikolo pamene anakumana na mavuto ? Mukanakhala Toñi , kodi mukanacita ciani ? ( Yos . 7 : 1 - 9 ) Inde , mpake kuti Yoswa anafunikila cilimbikitso . Kodi colinga ca Yehova cidzakwanilitsika bwanji ? Zimene simucita bwino : Kodi ni makhalidwe ati amene nifunika kuongolela ? Abulahamu anacita pangano ndi Eliezere lakuti sadzatengela Isaki mkazi pakati pa akazi acikanani . 1 : 14 , 15 ) N’zoonekelatu kuti iye anali kulakalakabe kupenyelela zamalisece . M’pomveka kuti makolo a Blossom , amene tam’chula m’ndime yoyamba , anali kufuna kutsimikizila ngati mwana wawo anali wokhwima mokwanila cakuti n’kumvetsetsa kuti kubatizika n’kofunika ndiponso ni nkhani yaikulu . Kodi cikumbumtima cimatithandiza bwanji kukhwima mwauzimu ? Kodi tingakulitse bwanji luso la mmene timaseŵenzetsela Mau a Mulungu ? N’ndani Akutsogolela Anthu a Mulungu Masiku Ano ? SIKUDZAKHALANSO MATENDA Colinga cabwino komanso cokhala na phindu lokhalitsa ni kutumikila Mulungu , na kuyesetsa kuthandiza anthu mwauzimu mmene tingathele . ” Coyamba yesetsani kukhala naye paubwenzi m’baleyo . Tsiku lina atate ananiuza kuti : “ Ukapita kukalalikila , usabwelenso . Ngati wothaŵayo wacoka mumzindawo , anali kuonetsa kuti sanali kudela nkhawa za moyo wa munthu amene anamuphayo , ndipo zimenezo zinali kuika moyo wake paciopsezo . Patapita nthawi yocepa , atumwi a Yesu anam’funsa kuti : “ Ambuye , kodi mubwezeletsa ufumu kwa Isiraeli pa nthawi ino ? ” — Mac . 1 : 6 . Kodi njila yabwino kwambili yothetsela zinthu zopanda cilungamo ni iti ? N’ciani cimene anapeza atafika kumeneko ? Mgwilizano ndi cikondi cao zinandikondweletsa kwambili . Nanga bwanji za mpingo wacikhiristu masiku ano ? Kodi Yehova amakufunila zotani ? Mofanana ndi atumwi aja , nthawi zina tingakhumudwe . Ndiye cifukwa cake amapewa kukhala na maganizo amphamvu ofuna kutsutsa zinthu zina zopanda cilungamo zimene boma lingacite . — Mat . Malinga ndi pangano la wansembe monga Melekizedeki , kodi mbeu idzacitanso utumiki wina uti ? Ndipo n’cifukwa ciani ? Poopa zimenezi abale anam’condelela kuti asapite . Ndili wosokonezeka maganizo conco , ndinayamba kudzidinda zizindikilo pa khungu , ndipo ndinayamba kumwa moŵa . Kutumikila pamodzi na anthu amene kale sin’nali kuwadziŵa , koma amene ali na cikhulupililo cofanana ndi canga , kwanithandiza kuona kuti palibe ciliconse m’dzikoli cimene n’cofunika mofanana ndi Ufumu wa Mulungu . ” David : Pambuyo pogwila nchito yovina kwa zaka zambili , ndinatopa ndi umoyo woyendayenda . Masiku ano , tili na zifukwa zambili zokhalila okhulupilika kusiyana na Yobu . N’cifukwa ciani umoyo ungakhale wovuta kwa anthu a Mulungu masiku ano ? Pofuna kuteteza moyo wake , Eliya anathaŵila kumwela m’dziko la Yuda ndi kupita ku cipululu copanda kanthu . — 1 Maf . ( b ) N’cifukwa ciani n’zosadabwitsa kuti nthawi zina timalefulidwa ? Mwamuna wam’nthawi zakale Yobu , anakumana ndi mavuto motsatizanatsatizana . Zimakhudza mtima kuona mmene makolo athu amavutikila ndi ukalamba . Popeza anali katswili wa zamaphunzilo , iye anayambitsa sukulu ku Nuremberg , ndipo ana a sukulu anali kuphunzila Ciheberi , Cigiriki , Cilatini , na Cijeremani kwa zaka zinayi cabe . Kwamveka kulila mofuula ndiponso momvetsa cisoni . Rakele akulilila ana ake . N’zoona kuti sitingapeweletu kulakwa kulikonse . Nthawi ina , mnzanga wa ku nchito ananiitana kunyumba kwake . Kodi ‘ anzathu ’ ndani ? Buku la cilamulo ca Mulungu litapezeka ndi kuŵelengedwa pamaso pa Yosiya , iye anayesetsa kugwilitsila nchito malangizo a Yehova . 3 : 1 - 6 ) M’kupita kwa nthawi , “ Yehova anaona kuti kuipa kwa anthu kwaculuka padziko lapansi , ndipo malingalilo onse a m’mitima ya anthu anali oipa okhaokha nthawi zonse . ” Iye anali ataona kuti atumwi ake sanali ogwilizana kweni - kweni . Pofuna kuwathandiza , ofesi ya nthambi m’dziko la Germany inakhadzikitsa dipatimenti ya zamalamulo pa Beteli mumzinda wa Magdeburg . Ndi mwai waukulu uti umene Mulungu watipatsa ? “ Pamene iye anali kukalamba , akazi ake anali atapotoza mtima wake moti iye anali kutsatila milungu ina . Sanatumikile Yehova Mulungu wake ndi mtima wathunthu monga mmene anacitila Davide bambo ake . ” ( 1 Maf . Way Koma anasoŵeka cinthu cofunika kwambili . Amene anapulumuka ndi Nowa , mkazi wake , ana ake atatu , ndi azikazi ao . M’masomphenya , mtumwi Yohane anamvela atumiki a Yehova a kumwamba akunena kuti : “ Ndinu woyenela , inu Yehova Mulungu wathu wamphamvu , kulandila ulemelelo ndi ulemu , cifukwa munalenga zinthu zonse , ndipo mwa kufuna kwanu , zinakhalapo ndipo zinalengedwa . ” NYIMBO : 61 , 52 N’ciani cinapangitsa kuti nchito yolalikila ibwelele m’mbuyo ku Britain ? Mwina tingafunse kuti : “ Tinene kuti mwana wanu wayamba kusamvela ndipo akucita zinthu zoipa kwambili , kodi mungacite ciani ? ” Tingaonetse bwanji kuti timakonda Yehova ndi ‘ zinthu zathu zamtengo wapatali ’ ? Yesu anali kulalikila “ uthenga wabwino wa Ufumu , ” ndipo afuna kuti ophunzila ake azicita cimodzimodzi . ( Miy . 14 : 17 ; 29 : 22 ) Komanso bwanji ngati munthu ali na nkhawa , kodi angapange zosankha mwanzelu ? ( Num . 32 : 6 - 12 ; Miy . ( Ŵelengani Mateyu 5 : 3 . ) Cifundo cake cinapatsa Aisiraeli okhulupilika mwayi woimabe zolimba ku mbali yake . A Zimba : Ehee ! Mau ake . Kuti zimenezi zitheke , mungadziikile zolinga pa mbali zitatu izi : ( 1 ) pa zikhulupililo zanu , ( 2 ) pa zocita zanu , ndi ( 3 ) pa mbali ya kukhala woyamikila . ( Gen . 5 : 28 , 29 ) Olo zinali conco , iye sanaike mtima wake wonse pa kufuna - funa cakudya , koma pa kucita cifunilo ca Mulungu . Ndipo ndinali ndi cidalilo coti azayankha pempho langa . Paulo analimbikitsa Akhristu a ku Kolose kuti : “ Monga ocita kusankhidwa ndi Mulungu , oyela ndi okondedwa , valani cifundo cacikulu , kukoma mtima , kudzicepetsa , kufatsa , ndi kuleza mtima . Conco , pamene anali kupumula anapemphela kwa Mulungu wake . Tifunika kudziŵa zimene zidzacitika cifukwa zidzatithandiza kuti tidzapulumuke . 38 : 16 ) Kodi n’ciani cidzacitika Gogi akadzaukila anthu a Mulungu ? ( Aefeso 4 : 13 ) Conco , dzifunseni kuti : ‘ Kodi ndimaŵelenga Baibulo tsiku lililonse ? Pamene Yesu anali padziko , Yehova anam’patsa mphamvu yocita zozizwitsa zomwe zinatsimikizila kuti amakondadi anthu . Inunso muli ndi udindo wothandiza ana anu kudziŵa Yehova ndi kum’konda . Kodi imwe pacanu mwaphunzilapo ciani zokhudza mdani wathu ? Molingana ndi asilikali ophunzitsidwa bwino , iwo ‘ amavala zida zonse zankhondo zocokela kwa Mulungu . ’ — Ŵelengani Aefeso 6 : 10 - 12 . Makhalidwe amenewa ndi ofunika kuti mudzakhale ndi banja lacimwemwe . ( Gen . 24 : 16 - 21 ; Rute 1 : 16 , 17 ; 2 : 6 , 7 , 11 ; Miy . ( Miyambo 14 : 23 ) Kodi kumapindulitsa bwanji ? Kristin anati , “ Kunali kuyamba kucita zimenezi , ndipo nchito imeneyi yatithandiza kupitiliza kutumikila m’dzikolo . ” Tsiku lotsatila , anthu okwana 2000 anatengako mbali pa nchito yolalikila ndipo ena anayenda mtunda wamakilomita 72 kucokela pamalo a msonkhano . Dzanja la manja kutanthauza inde ndipo dzanja la manzele kutanthauza ai . Ine n’natumikila kwa wiki imodzi na wadela n’kumaona mmene iye anali kucezetsela mpingo . Genesis caputa 24 - 27 Kodi n’ciani cina cimene tingacite pocilikiza ulamulilo wa Mulungu ? Hezekiya anakulila m’banja losiyana kwambili ndi la Rute . Koma Yesu anawadzudzula mwamphamvu . Kodi mau ake mwaaŵelengapo kangati , akuti : “ Monga mmene ucimo unaloŵela m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi , ndi imfa kudzela mwa ucimo , imfayo n’kufalikila kwa anthu onse cifukwa onse anacimwa ” ? Kaini akanasintha maganizo ake oipa , Yehova akanamuyanja . Si kuti umoyo wathu nthawi zonse wakhala wopanda mavuto . Kodi wamasalimo anatanthauza ciani pamenepa ? Ili na malangizo ocokela kwa Mlengi wathu . Coyamba , kumbukilani kuti Sebina anacotsewa pa udindo . * Koma zaka pafupifupi 20 m’mbuyomo , Mfumu Solomo analemba ndakatulo yokhudza mwamuna ndi mkazi amene analidi m’cikondi ceniceni . Akhiristu ena ‘ sanali kugwila nchito , koma anali kuloŵelela nkhani zimene sizinali kuwakhudza . ’ Ganizilani citsanzo ca Nowa . N’zoona kuti mabwenzi amene amatumikila Mulungu nawonso ni opanda ungwilo . N’zoonekelatu kuti palibe munthu amene angalepheletse dzanja la Mulungu . — Yesaya 54 : 17 ; ŵelengani Yesaya 59 : 1 . A Zimba : Ndiye kuti sindine ndekha eti ! Kodi cilengedwe cinali na ciyambi ? Kodi mumaganizila ena ? Mwacitsanzo , anthu mamiliyoni a ku Asia sadziŵa zimene Baibulo limakamba . Mau aciheberi amene agwilitsidwa nchito pa vesi limeneli amatanthauza “ phula ” zinthu zamadzimadzi zopezeka m’cilengedwe . Aisiraeli anali kudziŵa kuti kulambila mafano ni chimo lalikulu pamaso pa Yehova . ( Eks . Conco , citani zilizonse zimene mungathe kuti mupitilize kukhala pa ubwenzi wolimba na Yehova Mulungu ndi kugwilizana ndi gulu lake m’masiku otsiliza ovuta ano ! 24 : 14 ; 28 : 19 . Iyai . Yoswa sanabadwile mumzela wa mfumu Davide . Conco sanali woyenelela kukhala mfumu . Nthawi zina gulu limapanga masinthidwe . N’ciani cingaike ubwenzi wathu na Yehova paciopsezo ? Kwawo kwa Mairambubu ni ku dela lochedwa Naryn , m’dziko la Kyrgyzstan . Si tonse amene tingapite kumalo osoŵa kapena kuphunzila cinenelo cina . Anthu a m’dzikoli ali na maganizo olakwika pa nkhani ya cikondi . Kukamba zoona , tiyenela kuyamikila kuti Yehova anaseŵenzetsa mzimu wake woyela kuti tiphunzile coonadi ndi kulabadila uthenga wabwino . Itiphunzitsa kuti sitiyenela kulekelela abale athu akuvutika ngati pali zimene tingacite kuti tiwathandize . — Akol . M’dzikoli anthu ambili ni aukali . ( Yobu 31 : 32 ; Filim . 16 : 32 ) Munthu afunika kucita khama kuti akhale wodziletsa , monga mmene analili Yesu Kristu , munthu wamkulu woposa onse amene anakhalako . M’dziko lina , apabanja ena anali kuuza abale ndi alongo kuti azidya cakudya cinacake copatsa thanzi . Ndinagwilizana ndi gulu la acinyamata amene anali kukonzekela kuolokela tsidya lina la Nyanja ya Atlantic . A Yohane : Pali bwino . 96 : 1 . Kodi M’bale Diehl anacita bwanji ? Kuti aonetse kuti mau amenewo analidi oona , Yesu anayandikila manda ndi kufuula kuti : “ Lazaro , tuluka ! ” Nthawi zonse , mudzakhala woyamikila kwa munthu ameneyo cifukwa cakuti anakupulumutsani . Anthu amene n’nayamba nawo giledi 1 na amenenso n’natsiliza nawo sukulu . Anthu ambili a m’tauniyo n’nali kuwadziŵa maina awo , ndipo nawonso anali kunidziŵa . Timafunikiladi cilimbikitso monga cimeneci pamene tiyembekezela kukwanilitsika kwa malonjezo a Yehova . — 2 Pet . Posapita nthawi , nili na zaka 17 , n’nayamba kutumikila monga mpainiya . Koma mwacionekele anazindikila kuti ulosiwu umapeleka ciyembekezo cakuti anthu adzapulumutsidwa m’tsogolo . Conco , amakamba kuti Satana ayenela kuti anayesa Yesu m’masomphenya . Iye atakhala pa mbali pa mtembowo , anapemphela . Yehova anaganiza zakuti asawononge mtundu wonse wa Aisiraeli . ( Ŵelengani Mateyu 16 : 24 . ) Mu 2014 , Mboni za Yehova ku Myanmar zinali na msonkhano wacigawo wapadela . Inde , tifunika kumanga zolimba lamba ya ‘ coonadi m’ciuno mwathu ’ nthawi zonse . Anthu a Mulungu m’maiko osiyana - siyana , komanso a mitundu yosiyana - siyana amasonkhana pa malo olambilila padziko lonse lapansi . Ena amaganiza kuti afunika kuphunzila Ciheberi ndi Cigiriki kuti azitha kuŵelenga Baibo m’cinenelo cakale . Zozizwitsa za Yesu zimatithandizanso kudziŵa bwino umunthu wake ndi wa Atate ake . kukhululuka kwa Yehova ? Kuonjezela apo , iye amavutika kumva ndipo amayendela pa njinga ya olemala . Anthu ambili amene amaŵelenga mabuku athu si a Mboni za Yehova . ( 2 Tim . 4 : 18 ) Paulo anadziŵa kuti ngakhale kuti thandizo limene anthu angapeleke lingakhale losakwanila , thandizo limene Yehova ndi Mwana wake amapeleka limakhala lokwanila . Poyamba , sitinamulole . Ali ndi Avi , mwamuna wake Mulungu anatidalitsanso ndi mwana wamkazi wokongola amenenso amadziŵa Yehova ndi kum’konda . Kenako anauza makolo awo kuti ayende njila yozungulila boda kuti akakumane nawo kutsogolo . Koma kumisonkhano , akulu anandiuza kuti Amai akamauza acibale ao za ine ndiye kuti akulalikila kwa acibalewo . M’sonkhanowo unayamba na nyimbo zotamanda Mulungu . Pambuyo pake , M’bale Joseph F . 34 : 8 ) Anakambanso kuti : “ Yehova ni Tate wanga komanso Mnzanga wapamtima , ndipo umoyo wanga watsopano wanithandiza kum’dziŵa bwino kwambili . ( Mat . 16 : 6 , 11 , 12 ; Luka 12 : 1 ) Motelo , kunali koyenela kuti Yesu anagwilitsila nchito mkate wopanda cofufumitsa kuimila thupi lake lopanda ucimo . ( Aheb . ( Lev . 19 : 17 , 18 ; Aroma 3 : 11 - 18 ) Kodi mugwilizana ndi malangizo ake ? Kodi iye anavomeleza zimene olemba Baibo ena anauzilidwa kulemba za tanthauzo la cikhulupililo ca Mkhiristu woona ? Anapanga malamulo a zacilengedwe ndi okhudza makhalidwe abwino , pofuna kuti zinthu zonse zizicitika mwadongosolo . Panali acibale ambili amene ananilimbikitsa kuyamba upainiya . Buku lina linakamba kuti m’mbili ya anthu , palibe nthawi yaitali imene anthu anakhalapo pamtendele kuposa nthawiyo . Zimene Yesu , Mwana wacifundo wa Mulungu anakamba na kucita pamene anali padziko lapansi , zinaonetsa bwino cifundo cimene Yehova ali naco . ( Yoh . Sininafune kukangana naye koma n’naona kuti sanacite bwino ndipo n’nakhumudwa kwa ka nthawi . Kodi mumaona kuti ndinu woyandikana ndi Yehova ndipo mumam’dalila ? Posinkha - sinkha malingalilo a Mulungu , usana ndi usiku , ndi kuona mmene mfundo za m’Baibo zimathandizila , mudzalimbikitsidwa kwambili . N’cifukwa ciani Abulahamu anali kukhulupilila kuti Yehova amapeleka ciweluzo colungama nthawi zonse ? M’malo mwake , ndife otsimikiza mtima kuti zinthu “ zooneka n’zakanthawi , koma zosaoneka n’zamuyaya . ” — Ŵelengani 2 Akorinto 4 : 16 - 18 . Daniel anafotokoza kuti : “ Mkuluyo anandithandiza kuzindikila kuti ngati ndifuna kukhala wokhulupilika kwa Mulungu , ndiyenela kuleka kutumizila mtsikanayo mameseji . ( 1 Yoh . 4 : 8 , 16 ) M’kalata yake yaciŵili na yacitatu , iye anayamikila Akhristu amene “ akuyendabe m’coonadi . ” — 2 Yoh . 4 ; 3 Yoh . 3 , 4 . Si udindo wathu kuweluza anthu kuti ni oyenela kuwonongedwa kapena kupulumutsidwa . Mtsinje wa Kisoni unali kudutsa cigwa cimeneci kuloŵela Kunyanja Yaikulu ku Phili la Karimeli . ( Mateyu 28 : 19 , 20 ) Mlungu uliwonse , Mboni za Yehova zimathandiza anthu oposa 9 miliyoni kumvetsetsa Baibulo . yatsopano . Kodi angabwelele ndi kukawatsanzika komaliza ? ( Ŵelengani Ekisodo 4 : ​ 14 - 16 . ) Mwacitsanzo , ngati muli ndi ana , muli ndi nzelu zothandiza kwambili . Ndithudi , Baibulo limatilimbikitsa kugwila nchito mwakhama . Ganizilaninso cisangalalo cimene tidzakhala naco polandila anthu mamiliyoni ambili amene adzaukitsidwa . Tidzasangalalanso kuwaphunzitsa njila za Yehova ndi zimene iye wakhala akucitila anthu . ( Yes . 65 : 21 , 22 ; Mac . ( Mat . 5 : 12 ) Atumiki ena a Mulungu adzalandila mphoto yakumwamba . Ndipo ena adzalandila mphoto ya moyo wamuyaya m’paradaiso padziko lapansi . Akristu sabweleza pemphelo lacitsanzo la Yesu , koma mapempho a m’pempheloli ali ndi tanthauzo kwa ife . Adani a Paulo anayesetsa kucititsa anthu wamba komanso akulu - akulu a boma kuti aukile atumwi . 5 : 7 ) Kodi io ndi otangwanika kwambili ndi moyo cakuti amalephela kuona zimene Mulungu akucita ? ( Mat . ( a ) Kodi Paulo anayelekezela Cikumbutso ndi ciani ? Nanga anapeleka cenjezo lotani kwa anthu amene amadya zizindikilo ? ( Ŵelengani Salimo 34 : 22 . ) Kodi amamvela bwanji tsopano pamene akutumikila kosowa ? ( Numeri 14 : 18 ) Limeneli linali phunzilo lofunika kwambili limene Eliya anaphunzila pambuyo popilila ulamulilo wa mfumu yoipa kwa zaka zambili . “ Ndikudziŵa bwino kwambili kuti Yehova adzazengela mlandu anthu osautsika . N’cifukwa cakuti mavuto a tsiku ndi tsiku angasokoneze mgwilizano m’banja . Mwina iye analephela kuzindikila macenjezo osonyeza kuti mtima wake wayamba kutengeka , kapena anali kungowanyalanyaza . [ Mau apansi ] Kuti mudziŵe zambili , onelelani vidiyo yakuti , N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo ? Yankho ipezeka m’buku imodzi - modzi ya m’Baibo ya Chivumbulutso . M’caputa cina m’bukuli , iye amachedwa “ Mau a Mulungu . ” Mu 1989 , Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova linakhazikitsa dipatimenti yatsopano ku likulu la padziko lonse n’colinga cothandiza omasulila Baibulo . Komanso atabwela padziko lapansi , anaseŵenzetsa ufulu wake kukana mayeselo a Mdani wamkuluyo . ( Mat . ( Ŵelengani Salimo . 86 : 12 . ) * Ifeyo tikamayesetsa kuyandikila Mulungu , nayenso amatiyandikila . Anthu ambili padziko lonse lapansi akhalapo ndi mtendele umenewo . Kodi inunso mufuna kupindula ndi malangizo a m’Baibulo amenewo ? Kudziŵa maina ao kumatithandiza kuona nkhani zokhudza umoyo wao kuti ndi zenizeni . Anaika cidalilo conse mwa Yehova , ndipo anali wokonzeka kukwanilitsa utumiki wake kulikonse kumene Yehova akanam’tumiza . Nditafika zaka 16 , ndinayamba kucita maphunzilo ovina apamwamba pa sukulu imeneyo . Pa sukuluyi m’pamene ndinadziŵila David . Bauer ) , — November - December Kudziikila zolinga mukali aang’ono ni cinthu canzelu . 4 : 31 - 34 . Nchito Yomanga . Ndipo n’zosadabwitsa kuti Yosefe anali munthu wolemela . — Mat . Ngakhale pamene anali kale mkati mwa ulendo wautali umenewu , anali nawo mpata kapena ufulu wobwelela ku mzinda wotukuka wa Uri . Ŵelengani Salimo 45 : 12 , 14b , 15 . Mwacitsanzo , Way , katswili wokonza zamagetsi , ndi mkazi wake Debra , a zaka za m’ma 50 a ku Kansas , anagulitsa nyumba yao ndi katundu wao wina ndi kusamukila ku Wallkill kukatumikila monga anchito a pa Beteli amene amayendela . 24 : 45 - 47 ; Chiv . Mandy , * amene anali kuphunzila pa sukululi , anali wa Mboni za Yehova . Tikayamba kutelo , mwamsanga tiyenela kucita mogwilizana ndi lemba la Hoseya 12 : 6 , limene limati : “ Ubwelele kwa Mulungu wako . Usonyeze kukoma mtima kosatha ndi cilungamo ndipo nthawi zonse uziyembekezela Mulungu wako . ” Iwo angacite izi pofuna kuthandiza mwanayo kuona kufunika kowamvela , na kumufotokozela kuti malamulo awo ni oyenelela ndiponso ofunika kuwatsatila . Iye analoselanso zimene zidzatsatilapo pamene anati : “ ‘ Pa tsiku limenelo , tsiku limene Gogi adzabwele m’dziko la Isiraeli , mkwiyo wanga udzatulukila m’mphuno mwanga , ’ watelo Yehova , Ambuye Wamkulu Koposa . ( Luka 21 : 24 ) M’bale Russell anaseŵenzetsa nthawi yake , mphamvu , ndi ndalama zake mopanda kaso kuti auzeko ena coonadi . ( Ŵelengani Miyambo 24 : 14 . ) “ Ndife ziwalo za thupi limodzi . ” — AEF . Afunika kuleka zilizonse zimene zingamugwetsele m’chimo , ngakhale zimene amazikonda ngako . Ndikamvela zakuti ena akupita patsogolo ndimalimbikitsidwa , ndipo zimakhala za panthawi yake . Atakumana ndi vuto la zacuma , anagulitsa bizinesi yake , nyumba yake , ndi zinthu zambili zimene banja lake linali nazo . Kodi misonkhano yakuthandizani bwanji kuti muzicita zimene mumaphunzila m’Baibulo ? Anthu tonse ndise a Yehova . Tifune , tisafune , munthu aliyense wa moyo amafunika kugwila nchito . Kodi inu mungalalikile nao ? Conco , cinthu cimodzi cimene tiyenela kucita kuti tilimbane ndi Satana ndi kupewa kunyada ndiponso kuyesetsa kukhala odzicepetsa . Timakondwela kwambili kudziŵa kuti ngati tikhulupilila nsembe ya Yesu , Mulungu adzatikhululukila macimo athu , ndipo tidzakhala ndi cikumbumtima coyela . ( Aheb . 32 : 8 ) Timayamikila kwambili kuti Yehova amatithandiza kukwanilitsa ulaliki wathu . [ Mau apansi ] Mwacitsanzo , ndinasankha kosi yophunzila Cingelezi . Koma pambuyo pake zinthu zinasintha . Nowa , Danieli , na Yobu anapeza nzelu zaconco . 45 : 1 ; 49 : 3 . Dziŵani cipembedzo ndi cikhalidwe cawo , ndipo muzipewa kucita zinthu zimene zingawakhumudwitse . 14 : 22 - 24 ; 2 Mbiri 12 : 1 - 4 . Kodi ophunzila a Yesu anapindula bwanji panthawi ya Mtendele wa Aroma ? Iye anawafotokozela kuti “ pa maziko a dzina lake , m’mitundu yonse mudzalalikidwa za kulapa kuti macimo akhululukidwe . ” 19 : 32 . Cigwa ca Ela N’ciani makamaka cimene tiyenela kuyamikila masiku ano ? Enanso amati ni malo a bata ni mtendele kumene kumakhala angelo na anthu abwino amene anafa . ( April 1 , 2012 ) ; “ Kodi Anthu Onse Abwino Amapita Kumwamba ? ” Yehova anauza Abulahamu za lonjezo lake mobwelezabweleza . Ndipo nthawi iliyonse imene anakamba naye anali kuonjezapo mfundo zina . Apanso Jairo anayang’anitsitsa dzanja lamanja la Atate . Kodi ndi mavuto ati amene ana angakumane nao posamalila makolo okalamba ? Nanga angapilile bwanji ? Caka ciliconse anali kunibweletsela nsapato zanyowani zoseŵenzela . Lipoti ina inati : “ Cimene capangitsa kuti mavuto acepekele n’cakuti anthu agwilizana zakuti akonze zinthu padziko . ” Mulungu anakamba kuti ngati anthuwo sadzamumvela , adzafa . Gayo ayenela kuti anali woyang’anila mumpingo , koma kalatayi siikamba mwacindunji zimenezi . Zimenezi zikusonyeza kuti Baibulo ndi lodalilika . — 4 / 1 , masamba 10 - 11 . Yehova watilemekeza kwambili mwa kutipatsa mwayi wothandiza pa nchito yaikulu imene ikucitika masiku ano . Ngati timakonda Yehova ndi abale athu , tidzacita zonse zimene tingathe kuti kusiyana zibadwa kusasokoneze mtendele pakati pa anthu a Mulungu . Analalikila anthu ambili ndi kugaŵila zofalitsa zoculuka . ( Mat . 3 : 1 - 6 ) Anthu amene anali kubwela kwa Yohane kudzabatizika anali kucita izi poonetsa kuti alapa macimo amene anacita posamvela Cilamulo ca Mose . Tsopano Mirjana na mwamuna wake akhala mu utumiki wa nthawi zonse kwa zaka zoposa 30 . Zinanitengela Nthawi Yaitali ( J . Iye anawalangiza kuti : “ Pelekani kwa onse zimene amafuna . Amene amafuna msonkho , m’patseni msonkho . . . 32 : 27 - 29 . Ngakhale n’conco , anthu amene anagonjetsa anthu okhala mum’zindamo sanafune kuulanda ndi kukhalamo monga mmene ena anaganizila . ‘ Kodi mnzanga wa m’cikwati nam’nena kangati pa zimene walakwitsa ? ( Ŵelengani Deuteronomo 7 : 12 , 13 . ) Ndipo kwa zaka 8 zoyambilila , iye anali kuweluza milandu ndi anthu ena . Kodi pamenepa Paulo anali kuwaphunzitsa mfundo yanji ? Njila yaciŵili yopezela mtendele wa maganizo ni kuŵelenga Baibo na kusinkha - sinkha . Ndiyeno , mukatsiliza kuŵelenga ndime kapena mutu uliwonse m’cofalitsa , imani pang’ono ndi kuganizila zimene mwaŵelengazo . M’malo mwake , io anam’patsa nchito yolondela minda yampesa yao . ANTHU AMBILI AMAONA KUTI MUNTHU AMAKHALA WACIMWEMWE AKAKHALA NA CUMA CAMBILI . Popeza tikukhala m’dziko loipa lolamulidwa na Satana , tonse timakumana ndi mavuto . ( 1 Yoh . Pothandiza ana , kodi Mkhristu afunika kukumbukila ciani ? Yoyamba , kudzicepetsa kudzatithandiza kuzindikila kuti sitidziŵa mfundo zonse za nkhani imene yacitika . Timoteyo anaona mwamunayo akuyenda kwa nthawi yoyamba . YEHOVA anatipatsa mphatso yamtengo wapatali pamene anatumiza Mwana wake wokondedwa , Yesu , kuti abwele padziko lapansi . ( b ) Kodi Mau a Mulungu anathandiza bwanji m’bale wina kusintha khalidwe lake ? Ngati zaconco zakucitikilani , dalilani thandizo locokela kwa Yehova ndi kwa anthu ake n’colinga cakuti musakamaniwe mphoto . — Ŵelengani Salimo 34 : 18 ; Miyambo 13 : 20 . A Dorothy naonso amene anataikilidwa wokondedwa wao , ndipo anakhala wamasiye ali ndi zaka 47 , anafuna kupeza mayankho pa mafunso okhudza imfa . Ana amaona zilizonse zimene timacita , olo pamene ise tiona monga kuti sanaone . ” — Nicole . Musaleke kutumikila Yehova cifukwa cakuti wina anakukhumudwitsani 9 : 19 - 23 ) Na ise tiyenela kuyesetsa kuona moyo mmene Mulungu amauonela . Zoonadi , Yehova ndiye cimake ca cikondi . ( 1 Yoh . Ndinali kufunitsitsa kudziŵa kumene atate anali . Upandu : N’zoona kuti mitundu ina ya upandu yacepako m’maiko ena . Koma mitundu inanso monga upandu wa pa intaneti , nkhanza za m’banja , na ucigaŵenga , zaculuka kwambili . Ndiyeno mfumuyo inauza mtsikanayo kuti anali wokongola kwambili , ndipo anam’lonjeza mphatso zambili . M’malomwake , anali kukhulupilila kuti Mulungu angamuthandize monga mmene angathandizile “ munthu wocita zinthu moganizila munthu wonyozeka . ” Ndinali kulila ndi kupempha Mulungu kuti anditumizile munthu wondithandiza kumvetsetsa Baibulo . Iye anakamba kuti : “ Tinali na cidalilo cakuti tidzakwanitsa utumiki umenewu . ( Yoh . 2 : 1 - 10 ; Luka 5 : 29 ) Pamene vinyo anatha pa phwando la cikwatilo , iye anasandutsa madzi kukhala vinyo . Iwo anasankha kusamvela Mulungu . Ndinali kudzifunsa kuti : ‘ Kodi apita kumwamba ? ( b ) Kodi mu Salimo 136 , muli mau olimbikitsa ati ? Mwacitsanzo , ganizilani nkhani yokhala woona mtima . Panayiota anasintha umoyo wake , pamene anapezeka pamisonkhano ya mpingo ku Nyumba ya Ufumu ya Mboni za Yehova . Pamene Yesu anali kucita utumiki wake pano padziko lapansi , ophunzila ake analinso kubatiza anthu . 7 : 9 , 13 , 14 ) Ifenso tiyenela kutsanzila citsanzo cao cabwino cimeneci . — Mat . Anapilila zinthu zoipa zimene atumiki ena a m’bwalo la mfumu anali kumucitila . ( Yobu 42 : 5 ) Komanso , Yehova ananena kuti zimene Yobu anakamba ponena za Mulunguyo zinali zoona . — Yobu 42 : 7 , 8 . Kwa zaka 30 Yesu anali kugwila nchito ya ukalipentala , ndipo sanali kuseŵenzetsa zitsulo zamakono . Athandizeni kuti azitha kufotokoza zimene amakhulupilila momveka bwino ndiponso mwaulemu . Ngati iye amaonetsa makhalidwe a mzimu wa Mulungu mwa kukonda mkazi wake na kum’komela mtima , mkaziyo adzam’lemekeza kwambili . Ine ndi mkazi wanga takhala m’banja pafupifupi caka cimodzi , koma si nthawi zonse pamene timagwilizana maganizo . Uthenga umene ophunzilawo anali kulalikila sunagwilizane ndi miyambo yaciyuda imene atsogoleli acipembedzo anali kuphunzitsa kwa zaka zambili . Ndinafunika kuyambanso kucita bwino kuuzimu ndi kukhalanso ndi banja langa . ” N’ciani cimene acinyamata amene analeledwa ndi makolo amene si Mboni ayenela kukumbukila ? Zaka 100 zapitazo , acinyamata mamiliyoni ambili anacoka kunyumba zao ndi kupita kukamenya nkhondo . Ndi zosankha zotani zimene timapanga zokhudza cithandizo ca mankhwala ? Patapita milungu yocepa , iye anayamba kuzoloŵela kukwela pa ngamila . Iye anaonetsadi kuti anali munthu wanzelu . Ndipo anali wosadziŵa Malemba . Njila zatsopano zosindikizila zofalitsa zatithandiza kulalikila kwa anthu ambili . Adziŵeni bwino ana anu — maganizo awo , mmene amvelela , ndi nkhawa zawo . Ine ndi Laurie tinayamba ulendo wopita ku Africa , m’mphepete mwa nyanja , kenako kuoloka Nyanja ya Atlantic kupita ku United States . Koma amaonabe kuti ayenela kupitiliza kulimbana ndi cofooka cake . m’buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni , lofalitsidwa na Mboni za Yehova , ndipo lilipo pa webusaiti yathu ya www.jw.org . “ INE NDACITITSA KUTI IO ADZIŴE DZINA LANU ” Komabe , cosangalatsa n’cakuti zinthu sizili conco . 3 : 12 ; 17 : 14 ; 21 : 2 , 9 , 10 ) Adzaseŵenza pamodzi ndi Yesu kuti ‘ acilitse mitundu ya anthu . ’ Zimenezi zinalimbitsa cikhulupililo cao . Monga Mfumu , iye adzagwilizanitsa anthu a mitundu yonse ndi kuthetsa mavuto onse a anthu . — Ŵelengani Salimo 72 : 8 , 12 - 14 . 3 Tizithetsa Mikangano Mwamtendele Kuyambila nili mwana kudzafika zaka 18 , zinthu ziŵili zinali zozika mizu mwa ine : Cikomyunizimu na cikhulupililo cakuti kulibe Mulungu . 4 : 2 - 5 ) Motelo , Mulungu anaika m’dzanja la Mose umboni woonetsa kuti uthenga wake unali wocokela kwa Yehova . Antonio anakamba kuti : “ Zithunzi zamalisece zili paliponse m’dzikoli , ndipo zikhoza kukhazikika m’maganizo . Ndiye cifukwa cake tifunika kukonzekela tsopano kuti tidzakhalebe okhulupilika kwa Mulungu ngakhale panthawi yovuta . Pa usiku wakuti maŵa Yesu adzaphedwa , iye anafotokozelanso atumwi ake mphatso zosiyana - siyana zimene zikanawathandiza kupitiliza kubala zipatso . Ambili a io anapitilizabe kutumikila Yehova mokhulupilika ndipo anapilila zizunzo ndi ziyeso . Kuli apainiya apadela 369 amene akutumikila pa zilumba zosiyanasiya zokwana 28 Kodi tiyenela kudabwa kuti anthu onse a Mulungu amakumana ndi mavuto amene angacepetse cangu cao m’nchito yolalikila ? Patapita zaka , munthu wina amene tinali kuphunzila naye tisanadziŵe cineneloco anati : “ Ndife okondwa kuti tsopano mukukwanitsa kukamba cinenelo cathu . Conco , Yesu anamuuza kuti : “ Ukabwelela , ukalimbikitse abale ako . ” Malinga ndi zimene zili pa Salimo 45 , kodi “ anamwali anzake ” a mkwatibwi ndani ? Anafuna kuti Adamu na Hava ndi makolo onse azikonda ana awo , monga mmene Yehova anakondela ana ake aumunthu oyamba angwilo . Koma kodi Yosiya akanadziŵa bwanji kuti mau a Neko anali ocokela kwa Yehova ? Satana na ziŵanda amaseŵenzetsa maboma , cipembedzo conama , komanso anthu oyendetsa zamalonda ‘ posoceletsa dziko lonse lapansi kumene kuli anthu . ’ ( Chiv . Pemphelo silitipatsa cabe mwayi wopempha thandizo kwa Yehova , koma limatipatsanso mwayi womuyamikila . Yehova analenga zipatso ndi zakudya zina za mitundumitundu ndiponso zokoma kuti tizidya . Tikacita zimenezo , tidzakhala osangalala pouza ena zimene taphunzila . — Salimo 77 : 11 , 12 ; Luka 8 : 18 ; Aroma 10 : 15 . Nanga n’ciani cingatithandize kucita zimenezo ? M’malo mopita patsogolo ndi kukhala aphunzitsi , Aheberi anafunikila wowaphunzitsa . Nayenso Jason , yemwe anali kugwila nchito ku kampani ya zamagetsi , ndi mkazi wake Jennifer , a ku Illinois , anakamba kuti kugwila nchito yomanga pa Beteli ndi “ cimodzi mwa zinthu zosangalatsa kucita pamene tikuyembekezela dziko latsopano . ” Popeza Yehova amatidziŵa bwino , n’ciani cimene analonjeza ? ( a ) Kodi buku lochedwa codex linali ciani ? ( Yak . 1 : 14 ; 2 : 1 ; 4 : 1 , 2 , 11 ) Koma tikalakwa Yehova amatipatsa cilango , ndipo cilangoco cimakhala coŵaŵa . ( Aheb . Pa “ tsiku la ciweluzo ” la Mulungu , onse amene si mabwenzi ake adzaphedwa . Nchito yake inali yosiyana kwambili ndi imene anali kugwila kumwamba . Sitima imene m’Bale Russell anakwela yochedwa City of Chicago itayandikila tauni yochedwa Queenstown , iye anaona dzuŵa likuloŵa ca ku gombe la nyanja . 7 : 8 . ( Afil . 2 : 4 ) Pafupi - fupi aliyense amakondwela kuuzako anzake zokhudza umoyo wake . Zotsatilapo zake n’zakuti , tsopano onse m’banjalo akutumikila Yehova muutumiki wa nthawi zonse . ( a ) Fotokozani zimene zinapangitsa kuti Yesu acite cozizwitsa coyamba . ( b ) Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti ndi woolowa manja ku Kana ? Pamene anali kuona kuti iye anali kudalila kwambili Yehova , m’pamenenso io anali kumudalila kwambili . ( Yohane 11 : 11 ) Koma ophunzila a Yesu sanamvetsetse zimene anatanthauza , conco Yesu anawauza momveka bwino kuti : “ Lazaro wamwalila . ” — Yohane 11 : 14 . Kuciyambi kwa ulamulilo wake , Yehosafati analamula akalonga , Alevi , ndi ansembe kuti apite m’mizinda yonse ya Yuda kukaphunzitsa anthu Cilamulo ca Yehova . Cikondi na mgwilizano zinawonjezeka pakati pa ofalitsa . Nowa Ni njila zina ziti zimene tingaonetsele kuti timayamikila nchito yolalikila ? Yesu anabwela padziko lapansi na kufa “ kamodzi kokha . ” Ku Frankfurt , m’dziko la Germany , mu 1951 Yehova anali na colinga pouzila anthu kulemba nkhani zimenezi . ( 2 Tim . 4 : 10 ) Baibulo silichula mwacindunji zinthu za m’dziko zimene Dema anakonda zimene zinamucititsa kusiya Paulo . Koma m’dzikolo munabuka mavuto a zandale , ndipo tinasamukila ku South Vietnam . ( b ) Fotokozani mmene Bungwe Lolamulila lakhala likusiyanilana ndi Watch Tower Society . Yehova Amatisamalila ndi Kutiteteza , 2 / 1 Iye amaona zonse . Mwamuna wake anadabwa ndi kukamba kuti : “ Iyai , sindimakhulupilila zimenezo ! ” Pemphelo . Timaonetsa kuti timam’kondadi mwa kuika zofuna zake pamalo oyamba . M’kupita kwa nthawi Kristin anapeza makasitomala amene anali kugula nsomba nthawi zonse . Ndiponso , modzicepetsa tiyenela kuyendela limodzi ndi gulu la Yehova ngati pakhala kusintha kwa kamvedwe ka mfundo za m’Malemba . M’masomphenya a kumwamba amenewa , Danieli anaona angelo ambili - mbili . ( 1 Yoh . 4 : 8 ) Kodi ndi cikondi cimene anthu a m’banja limodzi amasonyezana ? Koma , mungafunike kupatulako nthawi ina mwa nthawi imene mumagwilitsila nchito posamalila maudindo ena kuti muphunzitse abale ena . ( Mlal . 19 : 16 - 19 ) Pa cocitikaco , Yehova anauza Aisiraeli kuti iye ni ‘ Mulungu wofuna kuti anthu azidzipeleka kwa iye yekha . ’ Inde , kudzidziŵa bwino kumeneko kudzatithandiza kudziŵa mocitila zinthu , kapena mokhalila ndi anthu ena . Nkhuku ndi anapiye “ Anthu ena anali kunditsutsa kaamba ka kuphunzila Baibulo . ▪ Kristu Ndiye Mphamvu ya Mulungu Kodi anamwino aŵili aciheberi anaonetsa bwanji kulimba mtima ? Masiku ano , kulibe Mwana wa Mulungu kuti atitonthoze mwacindunji . Paul , mwamuna wa ana aŵili anati : “ Ndalama ya m’dziko lathu itacepa mphamvu , zakudya zinakhala zodula ndiponso zosoŵa . ( Dan . 7 : 13 , 14 ) Posacedwa , Ufumu umenewu udzacotsapo mavuto onse . Komabe , galasi ingatithandize kuona maonekedwe athu kokha ngati tiiseŵenzetsa bwino . Iwo aphunzila kuseŵenzela pamodzi mogwilizana ndi mwamtendele . Anali atayelekezela mosamala ziphunzitso za machechi ambili , kuphatikizapo zipembedzo zina zosakhala za Cikhiristu , kuti aone ngati zinali kugwilizana na zimene Baibo imaphunzitsa . Mungamve bwanji mutamva kuti iye anaitaya kudzala kapena m’bini , kapena kuti anaigwilitsila nchito kuvulaza munthu wina ? Conco , m’pomveka kunena kuti dipo ndi umboni waukulu wakuti Mulungu amatikonda kwambili . Koma m’baleyo anapitilizabe kulalikila ndipo anaona mmene uthenga wa Ufumu unagonjetsela zopinga zazikulu . ( a ) Fotokozani zimene zinacitika pamene m’bale wina anali kulalikila . ( b ) Fotokozani zocitika za mu ulaliki zimene zinakucititsani kutsimikiza kuti Mau a Mulungu ni amphamvu . ( 2 Mbiri 14 : 12 , 13 ) Nthawi zina cifukwa ca dzina lake , Yehova anali kuthandiza ngakhale mafumu amene anali osakhulupilika kwa iye . ( 1 Maf . Linalembedwa Bwanji ? Mumayewa kukamba naye , kumukumbatila , kapena kuseka naye . ( Deuteronomo 21 : 22 , 23 ) Zikuoneka kuti Ayuda anali kutsatila lamulo limeneli ngati anthu apacikidwa pamtengo ndi Aroma . Munthu wokaikila Baibo angakufunseni kuti , Kodi mungaseŵenzetse kabuku ka malangizo a kompyuta yacikale - kale , kuti mudziŵe moseŵenzetsela kompyuta yamakono ? ( b ) Kodi nchito zimene Mulungu amapatsa atumiki ake zili ndi zotsatilapo zotani ? Mlongo Etta anam’thandizako Angela akali watsopano m’coonadi . Ngati ndi conco , mungafunike kulalikila mwakhama ngakhale pa nthawi imene anthu ambili amaona kuti ndi yopumula . Cifukwa cakuti anali kudya zizindikilo zimenezo mosayenelela Mulungu sanawayanje . Ngakhale kuti anali na zaka zambili conco , iye sanali okalamba kweni - kweni . Nditabatizidwa , ndinapitilizabe kusintha umunthu wanga . Zimenezi sizacilendo . M’maiko ena , ana aakazi amaonedwa kukhala osafunika , cakuti makolo amataya pathupi pa ana ambili aakazi . Atumiki a Mulungu amakhala ogwilizana : Mumpingo , timatsatila malangizo onse amene tapatsidwa . ( 1 Mafumu 16 : 31 - 33 ) Kulambila Baala kunali kuphatikizapo kucita miyambo yokhudza mphamvu ya kubeleka , kucita ciwelewele ndi kupeleka ana ao nsembe . Kusakhazikika pa zinthu zovutitsa maganizo M’bale Richard H . Kodi munthu “ wosalakwa ” ndani ? Ngakhale kuti ubatizo ni nkhani yaikulu , n’cifukwa ciani simuyenela kuopa kubatizika ? PA ANTHU Mu 1948 , mbale Nathan H . 4 : 6 , 7 , 13 . ( Mlaliki 9 : 11 ) Mu ulamulilo wa Kristu , anthu sadzavutika ndi mavuto alionse . — Miyambo 1 : 33 . Nditabwelela kwa makolo anga ndinali kuwaona mosiyana ndi mmene ndinali kuwaonela kale . ( Mateyu 18 : 10 ) Komabe , apa Yesu sanali kutanthauza kuti munthu aliyense ali na mngelo womuteteza , koma anali kungokamba kuti angelo amacita cidwi na wophunzila wake aliyense . “ Cilamulo ca Kristu ” : Ndi malamulo onse amene Yesu anapeleka , kuphatikizapo lamulo lakuti tilalikile uthenga wabwino padziko lonse , ndi lakuti tizikonda abale athu . MFUNDO ZIMENE TIYENELA KUKUMBUKILA Pa cikwati ca Mwanawankhosa , kodi mkwatibwi ndani ? Tiyenela kukonda Yehova kucokela pansi pamtima . Yesetsani kuphunzila Malemba amenewa kuti muziwakumbukila , cifukwa cakuti adzakuthandizani panthawi imene simudzakhala ndi Baibulo . Tiyamikila kwambili kuti cikondi cinacititsa kuti Yehova alenge cilengedwe conse ndi zinthu zonse zamoyo . KUTHANDIZA OSOŴA Anamuuza kuti : “ Ciliconse cimene ali naco cikhale m’manja mwako . ” 14 , 15 . ( a ) Kodi wacicepele amene afuna kubatizika ayenela kuganizila mfundo ziti ? N’ciani cingakuthandizeni kukumbukila ndi kumvetsetsa zimene mwaŵelenga ? 1 , 2 . ( a ) Kodi “ Mfumu yamuyaya ” ndani ? Nanga n’cifukwa ciani dzina limeneli n’lomuyenelela ? Paulo anaika maganizo ake pa mphoto yake ya moyo wosatha kumwamba . Ndipo nkhani imeneyi ikufika podetsa nkhawa . N’cifukwa cake timapitiliza kuwalimbikitsa kuphunzila coonadi ponena za Yehova na colinga cake kwa anthu . Mwakunena zimenezo , Yesu anaonetsa kuti Mulungu ndi wamkulu ndipo ali ndi mphamvu kuposa iye . ” M’nkhani ino ndi yotsatila muli mfundo zimene zingakuthandizeni . Mau a Mulungu amatilonjezanso kuti : “ Olungama adzalandila dziko lapansi , ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya . ” Ndi maganizo olakwika ati amene anthu ambili ali nao ? Kumeneko , Arthur anapeza abale angapo amene anathedwa nzelu , ndipo anali kungoyang’anitsitsa mkambi . Koma Eliya anamuthandiza mayiyo . Zimene Zingatithandize Kupeleka Yankho Zitsanzo zambili zimene zachulidwa m’nkhani ino zinatengedwa m’nkhani zakuti , “ Kuceza ndi Munthu Wina . ” Tizikonda adani athu . N’takumbukila zimene n’naphunzila m’Baibulo , n’nayamba kuona kuti Mulungu adzanilanga . Ukwati ungakhale wokondweletsa komanso mgwilizano wa moyo wonse . Conco , n’zoonekelatu kuti lemba la Chivumbulutso 21 : 4 limanena za madalitso amtsogolo pano padziko lapansi . — Sal . Zimene io amacita zimandicititsa kudzimva ngati ndikali wacinyamata . ” ( a ) Kodi Yehova ndi Tate wotani ? Onse anagwilizana ndipo sanali kuseŵenzetsa ndalama pa zinthu zosafunikila kwenikweni . Iwo akakumana na mavuto safuna - funa njila zothetsela cikwati cawo . “ Uci ndi mkaka zili kuseli kwa lilime [ la mtsikanayo ] , ” kutanthauza kuti mau ake ndi abwino ndiponso okoma ngati uci ndi mkaka . Kumeneko , Stephany amene panthawiyo anali na zaka 19 anakumana ndi Paul Norton mtumiki wa pa Beteli wacicepele . 10 TENGELANI CIKHULUPILILO CAWO | INOKI Iye akatiphunzitsa njila zake , ndipo ife tidzayenda m’njila zakezo . ” — Yesaya 2 : 2 , 3 . N’kutheka kuti Yesu asanabadwe ndiponso m’nthawi yake , Yehova anadalitsa akazi angapo ndi maudindo apadela . N’kutheka kuti mlongo wacikulileyo sanazindikile mmene mau ake analimbikitsila Marthe . Kumeneko kwangokhala kulephela kudziletsa . Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni Pamene anali ku Torowa , Paulo anaona masomphenya . Cinsinsi Namba 7 Makhalidwe Mofanana ndi anamwali anzelu amene anali okonzeka ndi nyali zao , odzozedwa akupitilizabe kuwala ndi kuyembekezela moleza mtima kubwela kwa Mkwati , ngakhale angaoneke kuti akucedwa . ​ — Afil . Kuonjezela pa kulimbana ndi ciyeso cimeneco , zinali kum’pweteka kuona anzake ena akukwatiwa mumpingo iye n’kukhalabe mbeta . Mwina Sisera anadutsa mumzinda umenewo pothawa , ndipo anthu a mumzindawo anali na mwayi womugwila koma anangomuleka . Mulungu amatisamalila mokoma mtima . Kudzela mwa Mose , Mulungu analangiza oweluza a Isiraeli kuti : “ Mukamazenga mlandu wa pakati pa abale anu muziweluza mwacilungamo . ” Timagwila nchitoyi modzipeleka cifukwa timakonda Yehova ndiponso anthu ena . Buku lina lofotokoza za mbili yakale linakamba kuti nthawi ya atumwi iyenela kuti inali nthawi yabwino kwambili ya Akristu kuyamba kulalikila , ndi kuti Akristuwo anaona kuti Mulungu anali atawakonzelatu njila . Zimawapatsanso mwayi wowonjezela utumiki wawo . Ganizilani mmene zinthu zinalili kwa mkazi wamasiye . Luca anakondwela kwambili cifukwa cakuti anakwanitsa kulalikila . 11 , 12 . ( a ) N’cifukwa ciani Mose ni citsanzo cabwino ca kulimba mtima ? Kukonda Yehova kudzatilimbikitsa kutengela citsanzo ca Yesu kapena kuti kutsatila mapazi ake mosamala kwambili . Ofalitsa nkhani amenewa amaonetsa kuti anthu olemela amene sagwila nchito zolemetsa ndiwo ali ndi “ umoyo wabwino . ” N’kutheka kuti m’dela limene timakhala , anthu amadziŵa kuti sititengako mbali m’ndale . 3 : 21 , 22 . 1 : 12 . 3 : 17 ) Izi zigwilizana ndi zimene anakamba Yesu m’fanizo lake la wofesa mbewu . Tikukhala m’dziko limene muli anthu odzikonda kwambili . Onse amene anali kumumvetsela , kuphatikizapo aphunzitsi , anadabwa “ ndi mayankho ake komanso poona kuti anali womvetsa zinthu kwambili . ” Ndithudi , Yesu molimba mtima anateteza coonadi copezeka m’Mau a Mulungu . Cifukwa ca khama lawo , uthenga wabwino unafalikila m’dziko lonse la Australia , ndipo unathandiza anthu ambili kuima kumbali ya Ufumu wa Mulungu . Conco , cina cimene cingakuthandizeni poimba ni kutsegula pakamwa kuposa mmene mumacitila pokamba . Mavuto akhoza kutifooketsa mwakuthupi na mwauzimu , ndi kuticititsa kukhala na nkhawa . 4 : 7 . Arthur ndi Nellie Claus anafika msanga pamsonkhano kuti apeze malo abwino okhala . Monique anafotokoza cifukwa cake . Dzifunseni kuti , kodi anthu anali ndi mphamvu zakuti angadziononge okha m’zaka 100 zapitazo ? Mulungu anayankha pemphelo lake mwa kutumiza mngelo amene anapha asilikali 185,000 a Asuri . — Yes . 3 : 2 , 3 ) Komabe , sanakwanitse kuthandiza Ayuda ambili kukhala olambila oona . Kaya tikuyembekeza kudzakhala ndi moyo wosatha kumwamba kapena padziko lapansi , tiyeni tikhale otsimikiza mtima kupitiliza kukhala okonzeka ndi kukhala maso . Janet akukumbukila kuti : “ Ndinali ndi nkhawa kwambili kaamba ka maudindo amene ndinali kufunika kucita . 9 Muzilimbikitsidwa ndi Mphatso ya Mulungu Yosatheka Kuifotokoza Yosimbidwa ndi Gerrit Lösch Ndithudi , Joachim anafunika kusintha maganizo ndi kulapa . Polembela kalata Akhristu a ku Tesalonika amene anali kukumana na cizunzo , iye anati : “ Popeza timakukondani kwambili , tinali okonzeka kukupatsani uthenga wabwino wa Mulungu . TSIKU lina pa Sondo m’maŵa , kuciyambi kwa caka ca 1520 , anthu a m’tauni ina yaing’ono ya Meaux pafupi na mzinda wa Paris , anadabwa kwambili na zimene anamvela m’chechi . Komabe , akapeza mpata , mkaziyo afunika kuwaphunzitsa coonadi anawo . Mwanjila imeneyi , amawathandiza kuti akule na makhalidwe abwino ndiponso kuti adziŵe Yehova . ( Mac . 9 : 26 . N’zosadabwitsa kuti patapita nthawi yocepa , akatswili a zacipembedzo pa Yunivesiti ya Sorbonne ku Paris , anayesa kuletsa Lefèvre kumasulila Baibo . Ndiye cifukwa cake mwamuna ndi mkazi amene akutumikila Yehova ayenela kukhala ogwilizana . Kanakamba kuti : “ Nifuna , koma siningapite cifukwa nilibe nsapato . ” Yobu anati : “ Zikanakhala bwino mukanandibisa m’Manda , . . . “ Mulungu akudziŵa zonse . . . . Yehova anali munthu weniweni kwa Ella monga mmene apolisiwo analili . Koma onani kuti Paulo atamvetsetsa coonadi cokhudza udindo wa Yesu pokwanilitsa colinga ca Mulungu , anacitapo kanthu . Cikhulupililo cathu cimalimba tikadziŵa makhalidwe a Mulungu osaoneka mwa kuona cilengedwe cake ( Onani palagilafu 17 ) Koma pali nkhani zina zimene palibe malamulo acindunji a m’Malemba . Nthawi zina , iwo anali kucita kugula udindo wokhometsa msonkho kwa akulu - akulu a boma na kuuseŵenzetsa kuti apeze ndalama zambili . Izi zatheka cifukwa ca khama la anthu a m’gulu la Mulungu logwilizana . “ Mngelo wa 7 analiza lipenga lake . Koma ndimadzimvela cisoni poona kuti ndinatenga nthawi yaitali ndisanapemphe kubwezeletsedwa . N’ciani cimene tiyenela kucita kuti tikonze cipulumutso cathu ? Timafunika kuulimbitsa “ nthawi zonse . ” Maulosi a m’Baibulo amatitsimikizila kuti zinthu posacedwapa zidzakhala bwino . N’zoona kuti munthu akapha mnzake mwangozi anali kumucitila cifundo . Kodi iwo anam’thandiza bwanji ? Iye analibe mwana , koma kupitila mwa mneneli Elisa , Mulungu anadalitsa mzimayiyo na mwamuna wake wokalamba mwa kuwapatsa mwana . Imodzi mwa mfundo zofunika kwambili zimene naphunzila mu umoyo wanga ni yakuti , “ zinthu zonse n’zotheka ” kwa Yehova . — Maliko 10 : 27 . Atsogoleli andale ndi abusa acipembedzo anali yakali - yakali kucilikiza nkhondo , koma Ophunzila Baibulo anali kulengeza za “ Kalonga Wamtendele . ” ( Yes . Mu September 2005 , ndinapatsidwa mwai wosayembekezeleka wotumikila m’Bungwe Lolamulila la Mboni za Yehova . ( 1 Mafumu 21 : 18 ) Yezebeli atauza Ahabu kuti munda wa mpesa tsopano ndi wake , Ahabu mwamsanga anapita ku mundawo . Pamene Yesu anali ndi zaka 12 , iye anaonetsa kulimba mtima pamene anali “ m’kacisi , atakhala pakati pa aphunzitsi . ” Makope oposa 1,600,000 a buku lochedwa Uthenga Wabwino wa Mateyu amatumizidwa m’mipingo ya ku Japan , ndipo ofalitsa amagaŵila makope masauzande ambili mwezi uliwonse . Ndipo pamaso pa Mulungu , anthu amenewa ni zitsanzo zabwino pa nkhani ya cikhulupililo na kumvela . — Ŵelengani Ezekieli 14 : 12 - 14 . N’cifukwa ciani mlongo Kristina anaona kuti afunika kusamukila mumpingo wacitundu ca m’dziko limene akhala ? Mfundoyo ni kukweza ucifumu wa Yehova na kukwanilitsika kwa colinga cake ca dziko lapansi . Zimenezi zidzatheka kupitila mwa Ufumu wake wolamulidwa na Khiristu , “ mbeu ” yolonjezedwa . — Ŵelengani Genesis 3 : 15 ; Mateyu 6 : 10 ; Chivumbulutso 11 : 15 . 5 : 6 , 7 ) Tiyenelanso kucita zimene tingakwanitse kuti tizipindula ndi misonkhano yathu na zinthu zina zauzimu . — Aheb . Mfundo zimenezi zimagwilanso nchito m’banja . 5 : 15 . A Zimba : Mukutanthauza ciani ? Conco , tili na cifukwa cabwino copitilizila kukhala pa ubwenzi wolimba na Mulungu . Baibo imakamba kuti : “ Wodala ndi munthu amene . . . amakondwela ndi cilamulo ca Yehova , ndipo amaŵelenga ndi kusinkhasinkha cilamulo cake usana ndi usiku . ” — Salimo 1 : 1 , 2 . Zitithandizanso kudziŵa mmene tingagwilitsile nchito mfundo zimene tidzaphunzila m’mafanizo amenewa pa utumiki wathu wacikristu . Kirsten anati : “ Mwamuna wanga ananithaŵa , n’kunisiya ndi ana anayi aang’ono . ” 2 : 5 , 6 . Yesu amene ndi Mfumu ya Ufumu wa Mulungu anayamba kulamulila pakati pa adani ake . Mwacitsanzo , Brian wa ku Britain analemba kuti : “ Nditafika zaka 65 ndinapuma pa nchito , ndipo izi zinacititsa kuti umoyo ukhale wosasangalatsa . Anthu anali pa cikondwelelo ca Pentekosite , cimene cinali kucitika kuciyambi kwa nyengo yokolola . Kodi Yehova ‘ amachela khutu ndi kumvetsela ’ ciani ? Komabe , “ palibe cilango cimene cimamveka cosangalatsa pa nthawi yomwe ukucilandila , koma cimakhala cowawa . ” N’tatulutsidwa m’ndende , n’nabwelela kwathu ku Karítsa . N’cifukwa ciani zimene Adamu na Hava anasankha kucita zinabweletsa mavuto ? Kodi cikumbumtima cathu cingatithandize bwanji mumpingo ? Kulambila kwa Pabanja — Zimene Mungacite Kuti Kukhale Kosangalatsa Kwambili 27 Ena angakhale ndi cizoloŵezi codziimba mlandu , ndipo ena cingakhale cifukwa ca mavuto amene amakumana nao . Yehova amakukondani inu panokha , komanso ali na cifundo ndi mphamvu moti angathe kukuthandizani pa mavuto anu . Popeza ndife ocimwa , sitingakhale na ciyembekezo ciliconse . Amuna na akazi amene ni okhulupilika m’banja mwawo amaona kuti cikwati ni mgwilizano wa moyo wawo wonse . Izi zimapangitsa kuti azidalilana . ( Gen . 3 : 1 - 6 ) Cifukwa cakuti anakana ulamulilo wa Mulungu , io anavutika ndipo anafa . M’malo mwake , iye anali kucenjeza Akristu odzozedwa za zimene zingadzawacitikile ngati atakhala oipa ndi aulesi . Ndi thandizo la Yehova , tinakhala pa ubwenzi wolimba ndi ana athu . ” N’taganizilapo mwakuya , n’naona kuti cili bwino nisapite ku sukulu koma niyambe nchito . Misonkhano yacigawo ndi yadela imaonetsa kuti Atate wathu wacikondi amadziŵa bwino mavuto athu ndi zosowa zathu . Pamene anali kumeneko , anali kucita zinthu momasuka ndi abale ake amene sanali Ayuda . “ Mphatso iliyonse yabwino ndi yangwilo imacokela kumwamba , pakuti imatsika kucokela kwa Atate wa zounikila zonse zakuthambo . ” Ayenela kuyesetsa kuwadyetsa bwino mwakuuzimu . Zina mwa nchito zimene Mulungu anapatsa Yesu ndi ‘ kumanga zilonda za anthu osweka mtima ’ ndi ‘ kutonthoza anthu onse olila . ’ 6 : 44 ) Popeza kuti Yehova wawakokela kwa iye , ndiye kuti amawaona kuti ni ofunika , ndipo amawakonda . Posacedwapa , padzikoli padzacitika mavuto amene sanacitikepo n’kale lonse . N’zolimbikitsa ngako kudziŵa kuti Yehova , Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , adzathetsa cisoni conse . Pamene ndinali ndi zaka 20 , ndinayamba kuphunzila Cimongoliya ndipo ndinakhala ndi mwai wocezela kagulu ka ofalitsa olankhula Cimongoliya . Iye anacita zinthu molimba mtima , anagwila nchito mwamphamvu , ndipo mothandizidwa na Yehova , anatsiliza nchito yomanga kacisi waulemeleloyo m’zaka 7 na hafu . Titangophunzilako mau ocepa ndi kuloweza pamtima ulaliki wacidule wogaŵila magazini , tinayamba kuyenda mu ulaliki . ( Yoh . 7 : 28 , 29 ) Nanga ndi zinthu ziti zimene mungacite kuti mulimbitse ubwenzi wanu ndi Yehova ? Iwo amaona kuti cilengedwe cimayendela malamulo odalilika , okonzedwa bwino ndi apamwamba . Motelo , kwa masiku angapo ndinali kugona m’galimoto yanga . Tiyeni tikambilane Cilamulo cimeneco kuti tione ngati “ njila [ za Mulungu ] zonse ndi zolungama . ” — Deuteronomo 32 : 4 . “ Pamene bwenzi lake lacisanu linapempha kuti ndiziphunzila nalo Baibo , ndinaona kuti ngakhale kuti ndili ndi zaka 65 sindiyenela kusiya kutumikila Yehova . Ngati timamvetsetsa zimene mau akuti “ Yehova Mulungu wathu ndi Yehova mmodzi ” amatanthauza , tidzam’konda ndi mtima wonse ndi kum’tumikila m’njila imene afuna . — Aheberi 12 : 28 , 29 . Timacita zimenezi pokwanilitsa mau a Yesu akuti : “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse . ” ​ — Mateyu 24 : 14 . Iye anauza azondi aciisiraeli kuti : “ Ndikudziŵa kuti Yehova akupatsani ndithu dziko lino . . . . Tinamva za mmene Yehova anaphwetsela madzi a Nyanja Yofiila pamaso panu . . . Tinamvanso za mmene munaphela mafumu aŵili a Aamori . ” Akristu oona amadziŵa kufunika kwa tanthauzo la dzina la Mulungu . Kuti akhale wathanzi , afunika kudya cakudya copatsa thanzi . 15 : 2 ) Kodi akapolo anali kukhala umoyo wabwanji kumeneko ? Mwina Yesu nayenso anamva conco pamene anali kukhomeleledwa pa mtengo wozunzikilapo , kunyozedwa ndi kumva ululu wosaneneka . N’cifukwa ciani sitiyenela kudabwa ngati malo athu m’gulu akusintha nthawi ndi nthawi ? “ Wauka kwa akufa . ” — MAT . Kuti muŵelenge Baibo m’zinenelo zosiyana - siyana pa intaneti kapena pa cipangizo canu ca makono , pitani pa www.jw.org . Olo kuti Rehobowamu anacita zinthu zina zabwino , sanapeze ciyanjo ca Mulungu . Kodi mukupita patsogolo mwa kuuzimu ? Mau oyamba a m’bukuli amafotokoza colinga ca ofalitsa bukuli kuti : “ Tikhulupilila kuti kuŵelenga bukuli kudzakuthandizani kukulitsa cidwi cofuna kuphunzila Baibulo . ” Popitiliza Mulungu anati : ‘ Ukacite zimenezi kuti akakhulupilile kuti Yehova . . . anaonekela kwa iwe . ’ ” ( Eks . Mwacitsanzo , taona kuti nthawi zokwanila 7 zikukhudza Ufumu wa Mulungu ndi kuti nthawi zimenezi zinayamba mu 607 B.C.E . Ngati taona kuti mapemphelo athu opempha thandizo sakuyankhidwa mwamsanga , tiziyembelekezela Mulungu amene amadziŵa nthawi yabwino yocitapo kanthu . Munthu amene Eliya anali kufuna ndi Elisa amene anali kulima ndi pulawo yomaliza . Anali kucita utumiki wopatulika modzipeleka na kuseŵenzetsa zimene anaphunzila kwa ena . N’cifukwa ciani dzina la Mulungu liyenela kupezeka m’Baibulo ? Davide anali kuŵeta nkhosa za atate ŵake kumapili a kufupi na Betelehemu . “ Ndinu woyenela , inu Yehova Mulungu wathu wamphamvu , kulandila ulemelelo ndi ulemu , cifukwa munalenga zinthu zonse . ” — Chivumbulutso 4 : 11 . Nsombazo zikathilidwa mcele , amayalapo mphasa pamwamba pake . 13 : 1 ; 29 : 21 . Yesu anali wozindikila kwambili . Kodi nchito yolalikila inawayendela bwanji ophunzila a m’nthawi ya atumwi ? Munthuyo anacoka mwamsanga popanda kuseŵenzetsa toiletiyo . Mavuto , Na . 15 : 13 ; Mac . 7 : 6 ) “ Zaka 400 ” zovuta zimenezo zinayamba mu 1913 B.C.E . pamene Isimaeli anayamba kuvutitsa Isaki . Ndipo zinatha pamene Yehova anamasula Aisiraeli ku Iguputo mu 1513 B.C.E . ( Gen . 21 : 8 - 10 ; Agal . Koma tinapitiliza nchito yathu , moti anthu ambili a kumeneko ni alambili a Yehova tsopano . Ndinayamba kucita upainiya m’caka comaliza ca maphunzilo a kusekondale . Baibo siiletsa kumwa moŵa pang’ono . Tidziŵa bwanji zimenezo ? ( 1 Maf . Yakobo anatuma ana ake kukagula cakudya ku Iguputo . Mayiyo anayankha foni na kufotokoza kuti mwamuna wake ali kunchito . Mu August 1523 , iwo analetsa anthu kumasulila Baibo kapena kulemba nkhani zokhudza Baibo m’zinenelo zofala . Iwo anali kuona kuti kucita zimenezo “ kungabweletse msokonezo m’Chechi . ” Anthu anali kumwalila msanga cifukwa ca matenda oyambukila kapena cifukwa ca ngozi . Pendani mwapemphelo ndi kuona ngati mumacita khama kuphunzila Baibulo . Kodi kuleza mtima kumaphatikizapo ciani ? Tinapindulanso cifukwa ca khalidwe lathu labwino m’njila zina . Masomphenya a namba 6 na 7 a Zekariya ni cenjezo lamphamvu kwa anthu amene amacita zinthu zacinyengo . Kwa zaka zambili , io akhala akulalikila uthenga wabwino wonena za tsogolo . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” — Machitidwe 20 : 35 . Atsogoleli amenewa sapanga ophunzila atsopano , koma amayesetsa kunyengelela mamembala ao kuti asawathaŵe . Azionanso kuti zimene umakhulupilila unaziganizilapo mozama . Pamenepo ana a Isiraeli anacita mantha kwambili ndipo anayamba kufuulila Yehova . ” ( Eks . Kumeneko , Mboni za Yehova zinapanga makonzedwe othandiza Mboni zinzao ndi anthu ena . Malo a Akazi m’Kakonzedwe ka Yehova ( Machitidwe 19 : 19 , 20 ) Pamene tinadzipeleka kwa Yehova , tinalonjeza kuti tidzayamba kucita zinthu zolemekeza Kristu pa moyo wathu . Pamene tipeleka cilango , tingatengele bwanji citsanzo ca Yehova na Mwana wake ? Mofanana ndi khoka limene silisankha , ndipo limasonkhanitsa nsomba zambili ndiponso “ zamitundumitundu , ” nchito yolalikila imakoka anthu ambilimbili a mitundu yonse . ( Yes . NJILA YOPEZELA CIMWEMWE Nanga anathandizidwa bwanji cifukwa cofeŵetsa umoyo wake ? Ayenelanso kuwatsogo lela mwacikondi makamaka akayamba kukaikila zinthu zina zimene timaphunzila m’Baibulo . — 9 / 15 , tsamba 18 - 21 . Iye anati mkaziyo “ waponya zoculuka kuposa [ olemela ] onse amene aponya . ” Cinanso , mudzaona kuti iye amatiuza za tsogolo labwino , nthawi imene tidzakondwela na “ moyo weni - weni ” kapena kuti moyo wosatha . Mulungu amafuna kuti tizidzimva kukhala otetezeka pansi pa ulamulilo wao . Atafika kumbali ina ya boda , makolowo anakumananso ndi ana awo ndipo anapitiliza ulendo wawo wopita ku msonkhano . Yesu anayelekezela nchito yolalikila uthenga wa Ufumu kwa anthu onse ndi kuponya khoka lalikulu m’nyanja . Makolo ambili amacita cidwi ndipo amatengako mabuku akuti Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa , buku loyamba na laciŵili , kuphatikizapo tumabuku twina . Koma kodi zimenezi zitanthauza kuti sitingathe kukondweletsa Yehova ? Pofuna kudziŵa zambili , n’nafunsa amayi kuti : “ Zingatheke bwanji Yesu kukhala Mwana komanso Atate pa nthawi imodzi ? ” Ndi kulankhulana kotani kumene kumalimbitsa ukwati ? Mtsikana wina dzina lake Rose anati : “ Ndimakonda Yehova ndipo ndimasangalala kutumikila Yehova kuposa kucita cinthu cina ciliconse . Ngakhale kuti pali maumboni ambili osonyeza kuti Ufumu wa Mulungu unakhazikitsidwa kale kumwamba , n’cifukwa ciani anthu ambili amakana kuvomeleza mfundo imeneyi ? 7 : 10 , 11 ) Ganizilani zimene Malemba amakamba ponena za anthu amene anali olapa na amene anali osalapa . Anakulila ku England kumene anayambila upainiya ali na zaka 18 . Inde , kupemphela ndi kusinkha - sinkha kunacititsa kuti cikondi cake pa Mulungu cikhale camphamvu kwambili kuposa cilako - lako cake cofuna kutamba zamalisece . M’masiku amenewo , ku Pine Bluff kunali mipingo iŵili , wina wa azungu na wina wa anthu akuda . 1 , 2 . ( a ) N’ciani cingatipangitse kufunsa funso lakuti : “ Mpaka liti ” ? Cifukwa Cake Baibulo Yapulumuka 8 * ( Aroma 12 : 12 ; Afil . 4 : 6 , 7 ) Onani mavuto amenewo ngati mwai wolimbitsa ubwenzi wanu ndi Yehova . Mngelo anauza Yosefe , tate wake wa Yesu kuti , Mariya wakhala ndi pathupi mwa mphamvu ya mzimu woyela . Yosefe wa ku Arimateya , Oct . Munthuyo anali kum’bwezela ku mzinda wothaŵilako kokha ngati apeza kuti sanaphe mnzake mwadala . ( b ) N’ciani cimene kholo liyenela kuona kuti ndiye cofunika kwambili kwa mwana wake ? Ndinali kuyembekezela kuti ndizisangalala ndi umoyo wa usisitele . Ndipo ngati nacita zinthu molakwitsako pang’ono , mwina nakwiya , kapena kukamba mau oipa , anali kufuula kuti : “ Ahaa ! Tiyenela kutsatila mfundo za m’Baibulo mwa kugwila nchito yosamalila Nyumba ya Ufumu kuti izioneka bwino monga malo olambilila . Yesu nayenso anavomeleza kuti kulalikila m’gawo la “ kwawo ” kunali kovuta . Mfundo imeneyi inalembewa m’mabuku onse anayi a Uthenga Wabwino . — Mat . Atate anathaŵa panyumba nikalibe kubadwa . ( Aefeso 5 : 25 ) Yesu anafika popeleka moyo wake cifukwa ca otsatila ake . Zimenezo zidzadalila mmene io amacitila zinthu ndi abale otsalila odzozedwa a Kristu amene akali padziko lapansi . ( 2 Timoteyo 4 : 9 ) Paulo anali kum’konda kwambili Timoteyo cakuti anali kumuchula kuti “ mwana wanga wokondedwa ndi wokhulupilika mwa Ambuye . ” Kodi mtsikanayo anacita ciani ? ( 1 Petulo 5 : 9 ) Zitsanzo za “ anthu amene anapilila ” zimatiphunzitsa mmene tingakhalile okhulupilika , zimaonetsa kuti nafenso tingathe kupilila , ndiponso zimatikumbutsa kuti tikakhala okhulupilika , tidzalandila madalitso . 10 : 12 ) N’cifukwa cake Paulo anapeleka cenjezo lakuti : “ Nkhawa yanga ndi yakuti mwina , monga mmene njoka inanamizila Hava ndi cinyengo cake , maganizo anunso angapotozedwe kuti musakhalenso oona mtima ndi oyela ngati mmene muyenela kucitila kwa Khristu . ” — 2 Akor . 3 : 2 ) Anthu ambili sayamikila zinthu zabwino zimene Yehova awacitila . Nayenso Atate wathu wakumwamba , Yehova , amatimvela tikamakamba naye kupitila m’pemphelo , umene ndi mwai wamtengo wapatali . Pambuyo popenyelela vidiyo yakuti , Young People Ask — What Will I Do With My Life ? , Sophie anati : “ Ndinazindikila kuti dziko linandipatsa cipambano ndi ulemu mosinthanitsa ndi utumiki wanga kwa Yehova . Kukamba zoona , nthawi zina nimavutika maganizo . Poyamba zinali zovuta kuti tipite patsogolo . Onani mmene Mau a Mulungu anam’khudzila . Paulo analangiza Timoteyo kuti : “ Kapolo wa Ambuye sayenela kukangana ndi anthu , koma ayenela kukhala wodekha kwa onse . Cifukwa cakuti nthawi yocepa kwambili imene timakhala ndi moyo imasiyana ndi mmene Yehova amaonela nthaŵi . Cimodzi mwa zolembazo , cimene papezeka dzina la munthu wochulidwa m’Baibo , ni kalata ya pangano la zamalonda imene inalembedwa mu 502 B.C.E . , caka ca 20 ca ulamulilo wa Dariyo Woyamba . Kodi ndili ndi ndandanda ya phunzilo laumwini ? N’ciani cathandiza Sheryl kupilila mavuto amenewa popanda kukhumudwa ? ( Ŵelengani Ekisodo 20 : 1 - 6 . ) Nayenso Yohane anatitsimikizila kuti : “ Ifetu timamudalila kuti ciliconse cimene tingamupemphe mogwilizana ndi cifunilo cake , amatimvela . ” Umphawi ndi vuto limene linayamba kalekale . Mwakuti anthu adzakomoka cifukwa ca mantha ndi kuyembekezela zimene zicitikile dziko lapansi kumene kuli anthu , pakuti mphamvu zakumwamba zidzagwedezeka . 15 : 11 ) Patapita zaka zambili , Yesu anakamba mau otsimikizila mfundo imeneyi . ( b ) Pankhani yomvela olamulila , kodi malile athu ni ati ? Komabe , Yesu anaonetsanso kuti cifukwa ca cizunzo , “ abale ” ake angasoŵe cakudya . Koma sizinathele pamenepo . Kodi mlongo wina anazindikila bwanji kuti Yehova amaona nchito zabwino zimene timacita ? Antonio anati : “ Atate atamwalila pa ngozi ya pamsewu , poyamba zinanivuta kukhulupilila . Tingaganize kuti , ‘ Mulungu akalibe kuniuzapo kapena kuuza mnzanga wa m’cikwati kucita ciliconse colinganako na zimenezo . ’ Aisraeli anamanga msasa m’mbali mwa phili limene linali kutsidya lina la cigwa . Kacisiyo anafunika kukhala ‘ wokongola , waulemelelo wosaneneka ndiponso wochuka ndi wotamandika kumayiko onse . ’ ( 2 Akorinto 13 : 5 ) Tiyeni tionetse kuti cikhulupililo cathu n’colimba mwa ‘ kulengeza poyela za cipulumutso , ’ kumatanthauza kulalikila uthenga wabwino . — Ŵelengani Aroma 10 : 10 . Mofananamo , pamene tigwilitsila nchito Baibulo kuti tidziŵe zophophonya zathu monga kudzikonda , sitifunikila kungoliŵelenga mofulumila kapena kuliŵelenga kuti tione zolakwa za ena . CAKA ciliconse , ophunzila Baibo masauzande ambili amabatizika . Baibulo ya Cingelezi ya William Tyndale inatetezeka ngakhale kuti atsogoleli ena anali kuletsa anthu kukhala ndi Baibulo , anali kuitentha , ndipo anapha Tyndale mu 1536 Lemba lina limene linan’thandiza ni Aroma 12 : 17 - 19 . Panthawi imene anali kukwanitsa zaka 15 , iye anali atatengela kale makhalidwe oipa a anzake . M’malo mwake , amapeleka nzelu “ moolowa manja kwa onse ” ndipo amatipatsa “ mphamvu yoposa yacibadwa ” kuti itithandize kulimbana ndi nkhawa zathu . — Yakobo 1 : 5 , 13 ; 2 Akorinto 4 : 7 . Kodi Akristu amene atumikila kwa zaka zambili angathandize bwanji acinyamata ? MFUNDO YA M’BAIBO : “ Nzelu yocokela kumwamba [ ndi ] . . . “ yopanda cinyengo . ” — Yakobo 3 : 17 . Pamene Rubeni anacokapo , abale akeo anaganizanso zomupha mnyamatayo , koma Yuda anapempha kuti amugulitse ku gulu la apaulendo m’malo momupha . Steffen , wocokela ku Denmark , anati : “ Tsiku lililonse , n’nali kulalikila anthu amene sanamvelepo za Yehova . 7 : 1 ; Aef . 5 : 3 , 4 ) Komanso , zimaphatikizapo makhalidwe oipa amene munthu angacite mseli , monga kuŵelenga nkhani zoutsa cilako - lako ca kugonana kapena kutamba zamalisece . Zimenezi zingalengetse munthu kuyamba cizoloŵezi coipa ca kudzipukusa umalisece . — Akol . Koma atate anga sanasangalale na zimenezi . Iwo ananiuza kuti , “ Ndiwe mwana , sufunika kulalikila . 5 : 32 ; 6 : 14 ) Nchitoyo iyenela kuti inaoneka yovuta kwambili cifukwa cingalawa cimene anauzidwa kuti amange cinali cacikulu . Ndipo uzimuyang’ana pamaso wapolisiyo . Kodi tifunika kupeza mayankho pa mafunso ati ? “ Cikondi n’coleza mtima ndiponso n’cokoma mtima . ” Ndiye kuti munthuyo sakukwanilitsa lonjezo lake kwa Yehova . Kuti tidziŵe amene akugwila nchito yolalikila masiku ano , tiyenela kuyankha mafunso anai awa : Tinali kukhala m’kacipinda kakang’ono kapamwamba m’nyumba ya matabwa ya nsanjika . Ndipo ngati mwakhala wofalitsa wa Ufumu kwa zaka zambili , ndi kwanzelu ndiponso kopindulitsa kuti muthandize kuphunzitsa atsopano “ Nyenyezi ” imeneyo inali ndi kiyi ya dzenje lolowela kuphompho ndipo inatsegula dzenjelo . Komabe , Yesu anacilikiza ulamulilo wa Mulungu mokhulupilika . Mwakugwilitsila nchito fanizo locititsa cidwi limeneli , Yesu anasonyeza kuti Yehova amafuna kuti anthu amene anasocela abwelele kwa Iye . Akristu okalamba amatengela kudzicepetsa kwa Yesu mwa kucilikiza acinyamata amene akutsogolela mumpingo ( Onani ndime 6 ) N’ciani cinacitika kwa m’bale wina atatengako mbali m’ndale ? Ndinafufuza kwa anthu ena ndipo anavomeleza kuti n’zoona . Koma ngati mulemekeza mwamuna wanu monga mutu wa banja , m’banja mwanu mudzakhala mtendele , Yehova adzatamandika , ndipo mwamuna wanu angakopeke n’kuyamba kulambila koona . Ndiyeno , nonse aŵili mungakhale na mwayi wokapeza mphoto . — Ŵelengani 1 Petulo 3 : 1 , 2 . Magazini ya The Golden Age inati : “ Mosakayikila , msonkhano umenewu udzakhala wosaiŵalika m’mbili ya Coonadi m’dziko la Mexico . ” Kodi m’cinenelo canu muli mabuku ocepa cabe ? Kodi Yesu anaonetsa ciani pamene analeketsa cimphepo ca mphamvu ? ( a ) N’ciani cimasonkhezela ophunzila Baibo masiku ano kuti abatizike ? Ndipo timamvetsetsa cimwemwe cao pamene zinthu zinawayendela bwino . Amaniuza kuti amanikonda ndi kuti amayamikila mmene napitila patsogolo kuuzimu . Ndipo pangano limene Mulungu anacita ndi Abulahamu lionetsa kuti Yehova ndi wofunitsitsa kukwanilitsa cifunilo cake cakuti anthu olungama ‘ adzaze dziko lapansi . ’ — Gen . Mapili a m’masomphenya a Zekariya ni olingana na mapili aŵili ochulidwa mu ulosi wa Danieli . Makhalidwe oyamba amene anachula ni cifundo na cisomo . Colinga cawo ni kulemekeza Mulungu mwa kucita cifunilo cake . ( 1 Sam . 10 : 2 ) Motelo n’kutheka kuti mau akuti Rakele analilila ana ake amatanthauza kulila kwake kophiphilitsa cifukwa ca kuphedwa kwa anthu a fuko la Benjamini kapena anthu a ku Rama . ( Aroma 5 : 17 - 19 ) Yehova anatsamutsa moyo wa colengedwa cake coyamba kucoka kumwamba kubwela padziko lapansi . ( Yoh . M’sitimayo munalinso Dr . Monga Wolamulila wa anthu , Yesu adzacita zinthu zabwino zambili . TSAMBA 9 Mwina mukusowa nchito , mumavutitsidwa ku sukulu , mukudwala , kapena muli ndi mavuto ena . Tinali kuyembekezela kuti adzatiyankha mwamsanga cifukwa woyang’anila cigawo wathu anali kufuna kuti tikacilikize mpingo wa ku Texas , tili monga apainiya apadela . Komabe , kubatizika kwa Yesu sikunali cizindikilo ca kulapa . ( Mat . ‘ Tulilani [ Mulungu ] nkhawa zanu zonse , pakuti amakudelani nkhawa . ’ Njila ina imene tingathandizile apainiya ndi mwa kugwila nao nchito mu ulaliki . Iye anati : “ Mau anu anandipeza ndipo ndinawadya . Panthawi imodzimodziyo Nowa anali “ mlaliki wa cilungamo . ” ( b ) N’cifukwa ciani timaphunzila Baibulo ? Cikhulupililo cathu cimatipangitsa kukhala olimba . Conco bwanji osayesetsa kukomela mtima ena mwa njila imeneyo ? — Aefeso 4 : 32 . Iwo anali kukonda kuimba nyimbo . Ndipo Mulungu anali kufuna kuti iye asamakayikile mfundo imeneyi . * Cidziŵitso cimeneci cathandiza anthu ambili kuleka cizoloŵezi cokoka fodya . ( b ) Kodi makolo mosadziŵa angakhumudwitse motani ana ao ? Komabe , anali kundilipilitsa ndalama zambili kaamba ka cinyengo canga ndi kugulitsa katundu popanda cilolezo . Ali mnyamata , iye “ anaphunzila nzelu zonse za Aiguputo . ” 20 : 12 ) Kodi n’ciani cinacititsa kuti ataye mwayi umenewu ? Mphamvu zanga zonse zinathelatu . . . Koma ena amaganiza kuti Mulungu amaseŵenzetsa cipembedzo kuti athandize anthu kukhala naye pa ubwenzi . Iye anadabwa atamvela kuti adzabeleka mwana mu ukalamba wake , cinthu cimene cinali cacilendo kwa iye . Conco , Sara anaseka mumtima mwake , akukamba kuti : “ Kodi mmene ndathelamu , zoona ndingakhaledi ndi cisangalalo cimeneci , komanso ndi mmene mbuyanga wakalambilamu ? ” Nthawi zina angelo anali kuonekela na matupi aumunthu kuti acite zimene Mulungu anawatuma padziko lapansi . Akatsiliza , anali kuvula matupi aumunthu na kubwelela kumwamba . — Oweruza 6 : 11 - 23 ; 13 : 15 - 20 . Musakhale cete pamene ine mtumiki wanu nikukhala wopanda covala . ” 1 : 8 ) N’cifukwa ninji Yesu anakamba kuti “ Mudzakhala mboni zanga , ” osati mboni za Yehova ? N’tacila , n’naleka kuseŵela m’timu ya akatswili . Mwacitsanzo , Yesu anati : “ Mukamakhululukila anthu macimo awo , inunso Atate wanu wakumwamba adzakukhululukilani . Koma ngati simukhululukila anthu macimo awo , Atate wanu sadzakukhululukilani macimo anu . ” Monga Timoteyo , ‘ muzisamala ndi zimene mumacita komanso zimene mumaphunzitsa . ’ — 1 Tim . Munthu wacifundo amasonyeza kuti ali ndi cikondi . Baibulo limakamba kuti “ akhwangwala ankamubweletsela mkate ndi nyama m’maŵa ndi madzulo , ndipo iye ankamwa madzi mumtsinje umene unali m’cigwaco . ” Conco , kuti tikhale monga Khristu , tifunika kudziŵa bwino maganizo na makhalidwe ake onse . Ndinali kuseŵenza pa cipatala cina m’dela la Boca Raton , ku Florida , ndipo ndinali kuseŵenzela m’cipinda ca odwala mwakayakaya . Tikatelo , Yehova adzakhala Bwenzi lathu mpaka kalekale . Nanga imakhudza bwanji mtima wathu ? ( b ) N’cifukwa ciani tinganene kuti ‘ Nyimbo yathu imanena za mfumu ? ’ ( 1 Akorinto 12 : 4 - 11 ) Koma patapita nthawi , kucita zozizwitsa kunatha monga mmene Baibulo limakambila . Tikamakonzekela Cikumbutso , tidzapindula kwambili kuganizila mwapemphelo za ciyembekezo cathu copatsidwa ndi Mulungu . Baibulo limakamba kuti Mulungu analenga munthu m’cifanizilo cake , kutanthauza kuti ndi wofanana ndi Mulungu . Kucita izi n’kupanda cikondi komanso n’kusowa ulemu . Njila zodzazidwa ndi anthu ku Yerusalemu pa Pentekosite mu 33 C.E . Mtumwi Paulo analemba kuti : “ Ndipo [ Khiristu ] anapeleka ena monga atumwi . . . . Kodi tingaphunzilepo ciani pa cocitika ici ? 3 Mmene Mungaipezele KUONONGEDWA KWA ZIPEMBEDZO ZIMENE ZALAKWILA MULUNGU NDI ANTHU . 4 : 16 ) Timasangalala ndi paladaiso wa kuuzimu , mmene timapeza cakudya ca kuuzimu ca mwana alilenji ndi ubale wacikondi wa padziko lonse . ( Mateyu 24 : 14 ) Kodi utumiki wathu ndi dalitso la Yehova kwa ena ? Atazindikila vutoli , anadziikila colinga cokhala mpainiya wa nthawi zonse , ndipo anayamba kuŵelenga nkhani za m’magazini athu zokhudza utumikiwu . Sara analidi wokongola m’makhalidwe , ndipo kukongola kwaconco n’kumene Yehova amaona kuti n’kofunika . Ndikulimbitsa . Ndithu ndikuthandiza . ” — Yes . 60,166 Anthu ananiseka cifukwa sin’nachoveko njuga wiki imeneyo , ndipo ananikakamiza kuti niyambenso , koma n’nakana . 10 : 39 ) Koma ise sitingaone zocita za Yesu mwacindunji . 3 : 27 . Ngakhale Yesu anakondwela na zakudya , ndipo anadyetsanso ena . Ella , amene akutumikila pa ofesi ina ya nthambi ya Mboni za Yehova mu Africa muno anati : “ Pamene ndinangofika pa Beteli , ndinaona monga sindidzakhalitsapo . Umu ndi mmene ndinafikila kunkhondo . Yehova na Yesu apeleka citsanzo cabwino kwambili pankhani yoonetsa khalidwe la cifundo . Mwacitsanzo , kodi cingacitike n’ciani ngati tipanga zosankha tili okwiya ? Mu 2011 , njila yatsopano yakuti Jairo azilankhulila inapezeka . ( Chivumbulutso 18 : 4 ) Koma kodi anthu a Mulungu anakhala liti akapolo a Babulo Wamkulu ? Anati : “ Undionetse cikhulupililo cako popanda nchito zake , ndipo ine ndikuonetsa cikhulupililo canga mwa nchito . ” ( Yak . Iye anavomeleza mwamsanga macimo ake ndipo analapa . Mavesi ambili m’Baibulo amaonetsa mmene moyo udzakhalila m’Paladaiso padziko lapansi . ▪ Mmene Akulu Angathandizile Ena Kukhala Oyenelela Maudindo Pamene Mike anali wacicepele anali kufunitsitsa kukatumikila ku dziko lina . 15 , 16 . ( a ) N’cifukwa ciani ena sangalandile uthenga wa Ufumu umene timalalikila ? Komanso anali “ kuyembekezela ufumu wa Mulungu . ” Mwina n’cifukwa cake anakhala wophunzila wa Yesu . ( Maliko 15 : 43 ; Mat . Ganizilani mmene munamvelela pamene munadziŵa kuti Mulungu ndi weni - weni ndi kuti mungathe kukhala naye paubwenzi wolimba . Kumbukilani citsanzo ca abale ake a Yosefe . Iye akukongoletsa kwambili gulu lake ndiponso paladaiso wauzimu amene tikusangalala naye masiku ano . Ganizilani funso ili , N’ciani cimacititsa munthu kukhala wacimwemwe ? Kuukitsidwa kwa Yesu kunasiyana motani ndi kuukitsidwa kwa anthu ena m’mbuyomo ? 22 : 17 ) Acinyamata ena amatsogoza maphunzilo a Baibo kuti athandize anthu kusangalala ndi umoyo wabwino . ( Yakobo 2 : 26 ) M’mau ena , munthuyo ayenela kukhulupilila Yesu , kutanthauza kuti ayenela kutsatila zimene amakhulupilila paumoyo wake . ( Aroma 7 : 22 , 23 ) Pemphelani kwa Yehova kuti akupatseni mphamvu . ( Phil . Siniona kuti n’nalakwitsa kucita zimenezi . Gulu Lake Ladongosolo Monga mwa Buku la Mau Ake , Nov . Koma iwo anaitenga mopepuka nkhaniyo . Muzikamba mau amene angacititse munthu amene mufuna kumuŵelengela lemba , kulemekeza kwambili Mau a Mulungu Mu 2003 , pambuyo potumikila m’Dipatimenti Yomasulila pa nthambi ya ku Fiji , ine ndi Jenny tinaitanidwa kuti kukatumikile m’Dipatimenti Yothandiza Omasulila ku Patterson , mumzinda wa New York . Motelo , tifunika kucita zonse zimene tingathe pom’tumikila . Mosakaikila , watsopanoyo adzapindula mwa kuona ndi kutengela njila zimene womuphunzitsayo akugwilitsila nchito mu utumiki . Tisanakambitsilane ndi munthu nkhani inayake ya m’Baibulo , tingacite bwino coyamba kudziŵa zimene munthuyo amakhulupilila . Kodi Jumpei amamvela bwanji pamene akutumikila m’gawo la citundu ca manja ku Myanmar ? Yesu asanapite kumwamba , anawapatsa nchito yocitila umboni “ ku Yudeya konse ndi ku Samariya , mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ” ( Mac . N’zodziŵikilatu kuti Yehova anaona nchito imene anagwila . M’bale John anakamba kuti pofuna kukwanilitsa colinga cimeneci , iye anasintha nchito kangapo konse kuti akhale na umoyo wosalila zambili . Aisiraeli anakhala pa mtendele kwa zaka 40 . Kodi zidzatheka bwanji kuti anthu akhalenso angwilo ? Umenewu unali mwayi wapadela wakuti acitile umboni molimba mtima kwa akulu - akulu a boma . Conco , cifukwa Yesu anakonda kwambili Atate wake ndi mbadwa za Adamu , iye anapeleka moyo wake nsembe . 4 ) Nanga ena angakuthandizeni bwanji kucita zimenezi ? Komanso , tingatengele makhalidwe oipa kwa anthu a m’dela lathu . Pokhala otsatila a Yesu , tiyenela kukhala maso kuti tiziteteze ku misampha imene ingationonge mwa kuuzimu . N’cifukwa ciani siniyenela kuloŵa m’tumagulu tolimbikitsa kusintha zinthu m’dziko ? ’ ( Eks . 5 : 2 ) Mwina anauzanso ana ao kuti pambuyo pakuti milili 10 yaononga Iguputo , ndi pamene Aiguputo analephela kugwila Aisiraeli pa Nyanja Yofiila , yankho la funso la Farao linayankhidwa bwino . Kodi kutengela zocita za Yesu kudzatithandiza bwanji kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova ? Iwo tsopano akugwila nchito ya m’dela . Timoteyo anali wophunzila wa Khristu amene anayamba kukonda coonadi ali wacicepele . Pokana milanduyo , Paulo anaseŵenzetsa Cilamulo ndi zolemba za aneneli . 4 : 16 ) Ngati tiphunzitsa anthu kupemphela m’njila yoyenela , kwa Munthu woyenela , ndi pa zinthu zoyenela , timawathandiza kukhala mabwenzi a Yehova , ndi kupeza thandizo akakumana ndi mavuto . — Sal . Baibulo likamanena za “ kulonjezedwa ukwati ” ndi Mkwati wakumwamba , amene ndi Yesu Kristu , mumadziŵa kuti likamba za inu , ndipo mumayembekezela mwacidwi kudzakhala “ mkwatibwi ” wa Kristu . ( 2 Akor . 11 : 2 ; Yoh . 3 : 27 - 29 ; Chiv . Zinthu zinasinthilatu mu umoyo wanga . ” Conco , “ cilango ” cimene Baibo imakamba , mbali yaikulu cimatanthauza kuphunzitsa , monga mmene makolo amaphunzitsila mwana wawo wokondedwa . Ngakhale n’conco , iye akanakhumudwa poona anzake akum’thawa . 14 , 15 . ( a ) N’ciani cimakucititsani cidwi na kuleza mtima kwa Davide ? NYIMBO : 141 , 134 Nkhani za anthu amenewa zimatikumbutsa mau ouzilidwa a mtumwi Petulo akuti : “ Mukavutika kwa kanthawi , Mulungu , yemwe amapeleka kukoma mtima konse kwakukulu , . . . adzamalizitsa kukuphunzitsani . Atacezela mipingo ya ku Galatiya , amishonale amenewo anacoka . Mngeloyo anayamba na moni . Anati : “ Mtendele ukhale nawe , iwe wodalitsidwa koposawe , Yehova ali nawe . ” Ndipo iye adzakuthandizani kuti mupitilize kum’tumikila ngakhale mukumane ndi mavuto otani . ( Yes . 55 : 7 ) Woipa aliyense payekha akalibe kulandila ciweluzo cake . Monga mmene Thomas anaonela , kuphunzitsa mwana kumafuna kuleza mtima . 14 : 1 ) Zimenezi zidzacitika panthawi inayake Gogi wa Magogi atayamba kale kuukila anthu a Mulungu . ( b ) Kodi alembi na Afarisi anapotoza bwanji Cilamulo ca Mulungu ? ( b ) Ni ufulu wa mtundu wanji umene anthu ali nawo ? Koma anakhala acangu ndi olimba mtima . Olemba Baibulo anagwilitsilanso nchito Cigiliki polemba malemba ena a m’Baibulo . MPHATSO yapadela imene tingalandile iyenela kutisonkhezela kuyamikila . Ndinali mwana wothela m’banja la ana 8 . Lili pafupi ndipo likubwela mofulumila kwambili . ” Iye afuna kuti tikhale ndi ‘ mtendele , ’ ‘ tsogolo labwino , ’ ndi ‘ ciyembekezo . ’ M’zikhalidwe zambili , zaciwelewele zinangokhala mbali ya umoyo wa anthu , cakuti zinaloŵelela mpaka m’miyambo ina ya cipembedzo . Ndinayambanso kukhulupilila Mulungu . Anzathuwa akali kulimbana na cizolowezi cawo ca kumwa moŵa mwaucidakwa ! ” ( Mat . 24 : 27 , 42 ) Kuyambila mu 1914 mbali zosiyanasiyana za cizindikilo cimene Yesu ananena zikukwanilitsidwa . Ngati nkhani ya kuukitsidwa kwa Yesu inali yopanda umboni , n’cifukwa ciani Petulo anaika moyo wake paciswe ? Raquel anafotokoza kuti : “ Pamene mwamuna wanga ananisiya mwadzidzidzi miyezi 18 yapitayo , n’nali na cisoni kwambili . N’ciani cimene anthu acita pofuna kuononga Baibulo ? Salmo 102 lionetsanso mmene mungakhalile ndi maganizo oyenela . Ngati n’telo , kumbukilani kuti Yehova sanapange anthu monga maloboti , amene saganiza kapena kupanga zosankha . Mofananamo , tifunika kuphunzila Mau a Mulungu tsiku lililonse kuti tidziŵe zimene Yehova afuna kuti ticite . Ndipo tikadziŵa , tifunika kucita zimenezo . Kuukitsa anthu akufa kumene Yesu anacita kunali umboni woonekelatu wakuti Mulungu anam’patsa mphamvu zogonjetsa imfa . ( Ŵelengani Salimo 16 : 10 . ) ( Onani cithunzi pamwambapa . ) ( b ) Nanga tikuyembekezela madalitso otani akuuzimu ? Popeza Yehova ni Wamphamvuyonse ndipo ni wanzelu zonse , palibe cingamulepheletse kukwanilitsa malonjezo ake . TIKUKHALA m’nthawi “ yapadela komanso yovuta , ” ndipo mavuto adzapitiliza kuwonjezeka mpaka pamene Yehova adzawononga dziko loipali na kubweletsa mtendele weni - weni . ( 2 Tim . [ 1 ] ( palagilafu 13 ) Onani buku la Gulu Lochita Chifuniro cha Yehova , mas . Jowana anali “ mkazi wa Kuza , kapitawo wa Herode . ” Kodi cikondi ceni - ceni cimatisonkhezela kucita ciani ? Popeza iwo aona zambili , angadziŵe zotulukapo za cosankha cinacake cimene tingapange na kutipatsa malangizo abwino . — Yobu 12 : 12 . 4 : 10 ) Kodi lembali litanthauza ciani ? Tifunika kupewelatu zovala zimene zingakhumudwitse ena . Baibulo limationetsa mmene tingakhalile ndi banja lacimwemwe ( Onani ndime 6 ndi 7 ) Baibo imakamba kuti tisamakondane “ ndi mau okha kapena ndi pakamwa pokha , koma tizisonyezana cikondi ceni - ceni m’zocita zathu . ” ( 1 Yoh . Komabe , kuti tikhale okhulupilika , tifunika kuikabe maganizo athu pa nkhani yaikulu imeneyi ndi kumvetsetsa kufunika kwake . Ngakhale n’conco , iye anaika maganizo ake pa zinthu zofunika kwambili , zimene ndi kucita cifunilo ca Mulungu . ( Yakobo 1 : 19 ) Tisanakambe ndi munthu , tingadzifunse kuti : ‘ Kodi iye angamvetsetse zimene ndifuna kukamba ? Pamene Mulungu anabweletsa cigumula kuti ayeletse dziko lonse lapansi , iwo anavula matupi awo na kubwelela kumwamba . Kungathandizenso wolakwayo kulapa na kupempha Yehova kuti amukhululukile . Iye afuna kuti tizigwilitsila nchito zimene timaphunzila ndi kuti tizithandiza ena . Mwacitsanzo , ku kilabu ina ya anthu ogontha ku Montreal , n’nalalikila wacicepele wina , Eddie Taeger , amene anali m’kagulu kenakake ka acinyamata ogontha . ( Luka 21 : 19 ) Cinthu ciliconse cimene munthu angacite sicingationonge kothelatu . Nanga panakhala zotulukapo zanji ? Comvetsa cisoni n’cakuti ena akalandila cilango , amakhumudwa . Izi zinacitika mu January , 1965 . Mtumwi Paulo anafananitsa mau akuti “ moyo wosatha ” ndi akuti “ moyo weniweniwo ” . Abale na alongo mu mpingo angalimbikitse acicepele mwa kucita zinthu zoonetsa kuti amawaona kukhala ofunika . ( 1 Akorinto 15 : 25 , 26 ) Ici ndi cifukwa cabwino kwambili cimene tiyenela kupemphelela kuti Ufumu wa Mulungu ubwele ndi kuti cifunilo ca Mulungu cicitike padziko lapansi . Cinanso , mungaphunzileko mau ocepa a m’citundu cawo amene angawakope cidwi . ( 1 Thess . 5 : 21 ) Mutu wa banja asanasankhe zocita pa nkhani inayake , afunika kupeza nthawi yofufuza m’Malemba ndi m’zofalitsa zosiyana - siyana zacikhristu , ndiponso kufunsa ena m’banja lake kuti afotokozepo maganizo awo . Ndi mavuto atatu ati amene ofalitsa osamukila ku maiko ena kumene kulibe ofalitsa Ufumu okwanila angakumane nao ? Ngakhale kuti anali oona mtima , kamvedwe kawo ka mfundo ya kugonjela maboma sikanali kolongosoka kweni - kweni . “ Kristu ndiye mphamvu ya Mulungu . ” — 1 AKOR . N’napita ku Beteli koyamba nili mnyamata wosakwatila . Pa nthawiyo , mu Philippines munali ofalitsa pafupi - fupi 10,000 . Kodi mungawapatseko malo okhala pa nthawi imene abwela kudzaseŵenza kapena kudzaona anthu ? — 3 Yoh . 5 - 8 . Inde , kupeleka moni wocokela pansi pamtima na kuyamikila ena kungalimbitse ubwenzi wathu na iwo . Ndiponso kumagwilizanitsa atumiki a Mulungu okhulupilika . Iye adzacitila cilungamo anthu osauka . ” Izi zingacitike cifukwa ndise opanda ungwilo . Tingayambe kudzifunila ulemu wopambanitsa . N’ciani cimakupangitsani kukhulupilila kuti Kristu adzagwilitsila nchito mphamvu zake kuthetsa mavuto padziko lonse ? Mvela mau ake , cifukwa amene adzachedwa mbeu yako adzacokela mwa Isaki . ’ ” Mu October 1974 , ndinayamba kulalikila nthawi zonse . Ndipo ndinali kuthela maola 100 mwezi uliwonse kuphunzitsa ena Baibulo . ( Mat . 2 : 13 , 14 , 19 - 21 ) Patapita zaka zambili , ophunzila a Yesu oyambilila “ anabalalikila m’zigawo za Yudeya ndi Samariya ” cifukwa ca cizunzo . ( Mac . Ine na mkazi wanga tili mu ulaliki ( b ) Kodi inu muyenela kutsimikiza mtima kucita ciani ? ( Aef . 4 : 31 , 32 ) Akhristu amene amayesetsa kuthandiza ena amakhala na cikumbumtima coyela , podziŵa kuti akucita zinthu mogwilizana ndi mfundo za Mulungu . Yesu anatiuza kucita zofanana ndi zimenezi pamene anakamba kuti : “ Ngati diso lako limakupunthwitsa ulikolowole n’kulitaya . ” M’malo moseŵenzetsa ufulu wathu ‘ kulimbikitsa zilakolako za thupi , ’ tifunika kusankha zinthu zotithandiza kulabadila cenjezo lakuti : “ Citani zonse ku ulemelelo wa Mulungu . ” — Agal . Mbuye anauza akapolo onse aŵili kuti : “ Wacita bwino kwambili , kapolo wabwino ndi wokhulupilika iwe ! Conco , anthu amene alandila ‘ mzimu wakuti akhale ana , ’ amachedwa ana a Mulungu a kuuzimu . Pamene anali kulalikila uthenga wabwino , iye anagwilitsila nchito mau abwino amene anadabwitsa omvela . Mwacitsanzo , panthawi imene Akristu a ku Tesalonika anali kuzunzidwa , Paulo anawalimbikitsa kuti : “ Pitilizani kutonthozana ndi kulimbikitsana monga mmene mukucitila . ” ( 1 Ates . Ni mafunso ati amene angatithandize kudziŵa ngati timam’kondadi Mulungu ? Nkhaniyi ifotokoza mmene tingapangile zosankha zabwino mwa kuganizila mmene Yehova Mulungu amaonela zinthu . ( Luka 11 : 13 ; Aheb . 4 : 12 ) Kuti nafenso tipindule na mphamvu imeneyi , tifunika kumaŵelenga Baibo tsiku lililonse , ndi kusinkhasinkha zimene taŵelenga . Asilikali a dziko la Japan analanda dziko la Philippines . Uthenga wotsatila wolembedwa pa mpukutu wouluka ni cenjezo lopita kwa anthu ‘ olumbila mwacinyengo m’dzina la Mulungu . ’ Lipoti lina mu Nsanja ya Mlonda linati , m’masukulu a sekondale ndi m’makoleji , “ aphunzitsi ndi ana a sukulu anacita cidwi ndi zithunzithunzi ndi malekodi puleya athu okondweletsa . 8 : 9 , 10 . Nanga anatiphunzitsa bwanji kuti kucitila anthu ena zaciwawa n’kulakwa ? Izi zitangocitika , Yehova anatuma Eliya kuti akakumane ndi Ahabu . Nthawi zambili munthu wocimwa amafunika kucotsedwa mumpingo kuti asinthe khalidwe lake . Umadziŵa bwanji kuti Mulungu alibe ciyambi ? ’ Kodi Ayuda Anali na Cizoloŵezi Canji Cimene Cinapangitsa Yesu Kuwaletsa Kulumbila ? Kutelo ndiko nzelu . Mumaganizila mmene mfundo zimene zikukambidwa zikumukhudzila ndi mmene zingasinthile umoyo wake . 15 : 23 ) Zocita zathu . Pita mu mtendele , matenda ako aakuluwo atheletu . ” ( Maliko 14 : 66 - 72 ) Nanga n’cifukwa ciani analimba mtima pamaso pa atsogoleli acipembedzo ? Baibo siphunzitsa kuti munthu aliyense ali na mngelo amene amamuteteza . N’nali kucoka panyumba usiku mwakazembela ndi kubwelelako m’mamaŵa kukali mdima . Msonkhanowu usanacitike , coonadi sicinali kupita patsogolo kweni - kweni ku Mexico . Kodi zimene takambilanazi zatiphunzitsa ciani ponena za mzela wobadwila wa Yesu , Mesiya ? N’zacisoni kuti amayamba kucita zinthu zimene ayenela kucita ndi mwamuna kapena mkazi wao cabe . Ngati n’conco , si inu nokha . Fotokozani zinacitika ndi Davide . Zikatelo , timadzimva kuti tili pa ubwenzi weniweni ndi Mulungu , ndipo timakhala ndi cikhulupililo ngati cimene Yesu anali naco pamene anati : “ Alipo ndithu amene anandituma . . . Kodi mpingo wa ku Efeso umafanana bwanji ndi atumiki a Yehova masiku ano ? Baibo imati : “ Mu Isiraeli munakhala cizolowezi cakuti , caka ndi caka ana aakazi a mu Isiraeli anali kupita kukayamikila mwana wamkazi wa Yefita wa ku Giliyadi , maulendo anayi pa caka . ” ( Ower . Aliyense wa ife angacite bwino kudzifunsa kuti : ‘ Pamene nitumikila Mulungu , kodi nimakonda kulekela ena kuti ndiwo azicita mbali yaikulu pa nchito ? Munthuyo ayenela kudzipeleka yekha ndi mtima wonse cifukwa cokonda Mulungu . Komabe , Yehova anaona cikhulupililo ca Abulahamu , moti anamuyesa wolungama . ( Aheberi 11 :⁠ 6 ) Mukadzipeleka kwa Mulungu ndi kubatizidwa , zinthu zidzakuyendelani bwino . Anthu osakhulupilika m’cikwati , a nsanje kwambili , ndi ongokaikila anzawo , anali kupatsidwa cilango . M’bale Hiroo atamva za kusoŵa kwakukulu m’dziko la Russia anayamba kuphunzila cinenelo ca Cirasha . 6 : 12 , 15 ) N’cifukwa ciani Abulahamu anafunika kukhala woleza mtima ? Yehova Amatsogolela Anthu Ake , Feb . Kodi m’mbuyomu munasintha zinthu pa umoyo wanu kuti muyambe utumiki wa nthawi zonse ? KODI munadzifunsapo kuti : ‘ Kodi Yehova angakonde kundipulumutsa pa cisautso cacikulu ? ’ Ni cuma citi cimene cimatipatsa cimwemwe ceni - ceni ? Citsanzo pankhani imeneyi ni mtumwi Paulo . Dzukani , fuulani mokondwela ! ” — Yesaya 26 : 19 . Mulungu analonjeza kuti mudzapeza cimwemwe ceni - ceni ngati muŵelenga , muphunzila , na kuseŵenzetsa zolembedwa m’buku ya ulosi imeneyi . — Chivumbulutso 1 : 1 - 3 . ( 2 Mbiri 15 : 1 , 2 ) Koma patapita zaka , Asa analephela kutsatila uphungu wabwino umenewo . Motelo makhalidwe a Mulungu ndiponso kacitidwe kake ka zinthu , monga zasonyezedwela m’Baibulo , ndi nkhani yofunika kwambili kuiphunzila . ” Onani “ Mafunso Ochokera kwa Owelenga ” mu Nsanja ya Olonda ya October 15 , 1987 . Nanga pangano la Cilamulo limafanana bwanji ndi pangano latsopano ? N’zoona kuti Goliyati anali wamtali mamita 2.9 , ndipo anali kuposa anthu onse , koma sanali kanthu poyelekezela ndi Mulungu wacilengedwe conse . Mwamsanga io akuloŵa mu Yerusalemu ndipo Ayuda opandukawo akuthaŵila m’kacisi . Nkhani Ya Pacikuto Komabe , ngakhale pambuyo pophunzila coonadi , ena mwa iwo anali akali kucita macimo aakulu . Yehova analamula Aisiraeli kuti asankhe mizinda itatu kum’maŵa kwa Mtsinje wa Yorodano , na ina itatu kum’madzulo kwake . 4 : 17 ) Motelo , m’nkhani ino ndiponso yotsatila , tikambilana zimene abalewa anafotokoza . Kapena munayamba kuona zinthu zina kukhala zofunika kwambili paumoyo wanu ? ( Akol . 1 : 16 ) Ponena za angelo amenewa , Baibulo limati : “ Panali atumiki okwana miliyoni imodzi amene anali kum’tumikila [ Yehova ] nthawi zonse , ndi atumiki enanso mamiliyoni 100 amene anali kuimilila pamaso pake nthawi zonse . ” ( Dan . Debora anali kukhala pakati pa mzinda wa Rama ndi Beteli m’dela la maphili la Efuraimu . N’naloŵanso kilabu ya zoyimba - yimba . Anali kudziŵanso kuti adzafa imfa yonyozeka . Nanga n’cifukwa ciani ? Baibulo limatikumbutsa kuti : “ Yehova amadzudzula munthu amene amam’konda , monga momwe bambo amadzudzulila mwana amene amakondwela naye . ” Ndiyeno , Suntuke nayenso anakonza maceza ake , n’kuitana abale na alongo amodzi - modzi aja , koma osaitana Eodiya . Ndilipo ndi moyo cifukwa cotsatila mfundo za m’Baibulo Popeza tili m’dziko limene anthu ake amaika zofuna zawo patsogolo , kodi citsanzo ca Sara si colimbikitsa kwa ise ? M’bale Mumba : Koma Mulungu anaonetsetsa kuti tidziŵe maina a anthu amenewa . 10 : 4 ) Amenewa ni makhalidwe a Mdyelekezi . 9 : 23 ) Cotelo , nthawi zonse tizionetsa Khalidwe Lopambana mu ulaliki . Cikumbumtima cathu tingaciyelekezele na kampasi . N’ndani amene Sara anali kudzasiya ? Kwa zaka 135 , kuyambila pamene Nsanja ya Mlonda inayamba kufalitsidwa , yakhala ikucenjeza aŵelengi ake kuti ulamulilo woipa wa Satana udzatha , ndipo udzaloŵedwa m’malo ndi Ulamulilo wa Zaka 1000 wa Yesu Kristu . — Chiv . Zikakhala conco , tingacite bwino kudzifunsa kuti , ‘ Kodi Yesu akanacita ciani pamenepa ? ’ Cikondi cao pa Yehova cinawathandiza kupanga cosankha ca nzelu . Pangano latsopano linayamba liti kugwila nchito ? N’cifukwa ciani ophunzila anali kugwilitsila nchito Cigiliki ? Nthawi zina mungalephele kukhala oleza mtima , koma panthawi yovuta imeneyi , muzikumbukila kuti kupeleka cilango mwaukali nthawi zambili kumakhala kwankhanza , kopitilila malile , ndipo kosathandiza . Baibulo limati panthawi imene Nowa anali ndi moyo , “ dziko lapansi linali litaipa pamaso pa Mulungu woona , ndipo linadzaza ndi ciwawa . Ndipo tagaŵila zofalitsa zambili padziko lonse lapansi . 11 : 20 - 24 ) Iye anali kukhulupilila kuti m’tsogolo , mlongosi wake adzauka . Monga Bezaleli ndi Oholiabu , timakhala okhutila kucita cifunilo ca Yehova podziŵa kuti iye akusangalala ndi nchito yathu . Ngati nchito yanu imakuthandizani kupeza ndalama zogulila zinthu zofunika , ndiye kuti ndi yabwino . ” ( a ) Kuyambila kale , n’ciani cimene atumiki a Mulungu amadziŵa pankhani yophunzitsa ena ? Ena amawononga nthawi yoculuka kuona mapikica a anthu amenewo kapena kuŵelenga nkhani zokhudza anthuwo . Mpingo wonse umafufuza anthu oona mtima . Ndife oyamikila kuti Yehova akutithandiza kupewa zinthu zoyambitsa magaŵano , kunyada ndi mpikisano zimene zafala m’dziko la Satanali . “ Tidzapita ise ! ” Conco , kudedwa cifukwa cocitila umboni za dzina la Yehova n’cimodzimodzi ndi ‘ kunyozedwa cifukwa ca dzina la [ Yesu ] Kristu , ’ amene anati : “ Ndabwela m’dzina la Atate wanga , ndipo simunandilandile . ” N’cifukwa ciani Akristu acikulile timawayamikila kwambili ? Ena anafika polandila maudindo m’gulu . Kucita zimenezi n’kofunika , ndipo Ufumu wa Mulungu umalimbikitsa nzika zake kukhala ndi makhalidwe amenewa . Kuposa pamenepo , Ufumu wa Mulungu umalamula nzika zake kukhala ndi makhalidwe abwino . Malinga n’zimene Baibo imakamba , tidziŵa kuti si nthawi zonse pamene Yehova amateteza atumiki ake mwakuthupi . ( Mac . Baibo imati : “ Mawu onenedwa pa nthawi yoyenela ndi abwino kwambili . ” Mwacitsanzo , sitiyenela kufunsa mkazi wa wodzozedwa kuti ; ‘ Kodi mumamva bwanji mukaganizila kuti m’dziko latsopano simudzakhala ndi amuna anu ? Atamasulila malotowo , Yosefe anatengelapo mwayi wofotokozela mnzakeyo za vuto lake . Patapita nthawi yocepa Yesu ataukitsidwa , anakumana ndi gulu la ophunzila ake oposa 500 . Lelolino , anthu ambili amanena kuti ndi Akristu , “ koma amamukana [ Mulungu ] ndi zocita zao cifukwa ndi onyansa ndi osamvela , ndipo ndi osayenelela nchito iliyonse yabwino . ” Ngati zingatheke , mukhoza kumawanyamulako pa motoka yanu popita kumisonkhano . Mwacitsanzo , kapeti ya Aperisiya ya m’zaka za m’ma 1500 ku Philadelphia Museum of Art ku Pennsylvania , m’dziko la America , anaikongoletsa mwa kusokelapo pikica yoonetsa munda wochingidwa wa mitengo na maluŵa . Ena adzapitilizabe kupilila masautso a mwakabisila mpaka m’dziko latsopano . Kale kwambili , magalimoto anali odula ku Japan ndipo miseu inali yoipa . 20 : 28 ) Mwacitsanzo , Yesu panthawi ina anasambika mapazi atumwi ake . Inde , muzicilikiza cilango ca Mulungu osati kucita zinthu motsutsana naco . ( Ŵelengani Miyambo 11 : 14 . ) Zolemba zakale zimene zinachulako za “ nyumba ya Davide na zimene Yesu anakamba , zimatsimikizila zimenezi . Kodi tiyenela kucita bwanji ngati m’bale wathu wakamba mau oipa kapena wacita zinthu zimene zatikhumudwitsa ? Koma ngati amaona kuti timawanyalanyalaza , angaleke kutiuza zinthu ndipo angapeze wina womuululila zakukhosi . ” — Maranda . Kukhulupilika kuli monga nangula , kumateteza cikwati canu m’nthawi zovuta Pa cifukwa cimeneci , masiku ano tili na mwai wokhala nayo ndi kuiŵelenga . Paulo anali citsanzo cabwino pa nkhani yotengela Mulungu ndi Mwana wake . Mwacionekele , palibe aliyense wa ise amene angafune kucita zinthu zimene zingasonkhezele m’bale wathu kuyambilanso khalidwe limene lingamuwononge mwauzimu . Anthu pafupi - fupi 70 miliyoni anafa ndi njala m’zaka za m’ma 1900 . Koma alambili okhulupilika amene anapatuka pa zinthu zoipa ndi kuleka kucita zosalungama anapulumuka . Yesu anati : “ Amene ali ndi malamulo anga ndipo amawasunga , ameneyo ndiye amene amandikonda . ( Aheb . 13 : 15,16 ) Conco mofanana ndi atumiki a Mulungu akale , nafenso tiyenela kuphunzitsidwa kuti titamande Mulungu mwa zocita zathu ndi kupambana pa nkhondo yathu yakuuzimu . ( b ) Nanga malembawo amatiphunzitsanji za Yehova ndi Mwana wake ? ( b ) Ni funso liti limene tingakambilane ndi anthu okondwelela ? ( Mika 7 : 7 ) Kwa zaka zambili , atumiki a Mulungu anali kuyembekezela kukwanilitsidwa kwa maulosi okhudza Mesiya kapena kuti Kristu . — Luka 3 : 15 ; 1 Pet . Kodi tingasoceletsedwe bwanji ndi “ cinyengo camphamvu ca cuma ” ? Zikutionetsanso kuti posacedwapa tidzaona zozizwitsa zambili zikucitika padziko lonse . Nanga zotsatilapo zake zinali zabwanji ? N’zacisoni kuti mkazi wanga wokondedwa Maria , anamwalila mu 2014 . Anthu pamsonkhanowo anali na cidwi cofuna kudziŵa tanthauzo lake . Milandu ina imene tawina yapangitsa makhoti ena kusintha malamulo awo . Izi zacititsa kuti tikhale na mwayi kapena kuti ufulu wa kulankhula ndi wolambila . ( Agalatiya 6 : 16 ; Machitidwe 3 : 21 ) M’masomphenya amenewo , mafupa anakhala ndi moyo , kenako anakhala gulu lalikulu lankhondo . Kumbukilani Yosefe . 12 Thandizo pa Kupilila Mavuto Makolo anga analinso okhumudwa ndi abusa a chechi ca Baptist , amene anali kungofuna zawo zokha . Yehova ni Mlengi wodabwitsa kwambili . Baibulo limati : “ Mwa cikhulupililo , anthu a Mulunguwo anaoloka Nyanja Yofiila ngati kuti akudutsa pamtunda pouma , koma Aiguputo atalimba mtima ndi kulowa panyanjapo , nyanjayo inawamiza . ” ( Aheb . Adani athu akuphatikizapo angelo oipa kapena kuti ziwanda . ( Chiv . Kodi kukhulupilila Yehova kunathandiza bwanji mlongo wina kupilila atakumana ndi mavuto ambili ? N’cifukwa ciani tumapepala twauthenga twatsopano n’tothandiza kwambili ndiponso tosavuta kugaŵila ? Paladaiso ameneyu angatanthauze Paladaiso weniweni wa padziko lapansi amene akubwela posacedwapa . Tisalole ndalama kapena katundu kusokoneza ubwenzi wathu ndi Yehova . Maria Victoria anali kukonda kunena anthu ena . Kodi Ophunzila Baibo anacita ciani molimba mtima , poonetsa kuti anaona kufunika kolekana ndi cipembedzo conama ? Kukumbukila mmene amasonyezelana cikondi kumathandiza cikwati cao kukhala colimba . Mabwenzi : Anthu amakondwela kuceza komanso kugwila nchito ndi anthu amene ali na zolinga mu umoyo wawo , amenenso amayesetsa kuzikwanilitsa . * Ciŵelengelo ca amene timaphunzila nao Baibulo cimaposa ciŵelengelo ca anthu m’maiko ena 140 paokhapaokha . Henri analimbikitsiwa na woyang’anila dela amene anapita naye ku lesitilanti kukamwa naye tiyi . Tinafunsa kuti zilembozo zinali kutanthauza ciani , koma zinaoneka kuti panalibe amene anali kudziŵa . Pambuyo pophunzila Baibulo kwa miyezi 5 ku New York , ine ndi anzanga ena atatu anatitumiza ku zisumbu zing’ono - zing’ono za pa Nyanja ya Caribbean . Zokamba za wansembeyo zionetsa kuti sindife opusa koma kuti ndife ogwilizana monga Akristu oona . Kodi ndikali kutumikila Yehova mwakhama ? ( Mlal . 12 : 1 ; Mat . Nthawi zambili , polalikila pa nyumba imodzi uthenga wa m’Baibo , anthu 5 kapena 6 apafupi amabwela kudzamvetsela . Anapeza kuti ndi amene tsopano akutumikila monga mgwilizanitsi wa bungwe la akulu . N’zoonekelatu kuti Yesu anali kudziŵa kuti munthu akamapemphela amakambadi ndi Yehova . Koma kuti inu mulandile madalitso amenewa , coyamba muyenela kudziŵa Mulungu ndi cifunilo cake . Cofunika kwambili kuti tikapeze moyo wosatha ni “ kudziŵa ” Yehova na “ kukhulupilila ” Yesu , Mwana wake wobadwa yekha . Tiyenela kuteteza umoyo wathu wakuuzimu ndi unansi wathu ndi Yehova . Cina , tiyenela kuika Ufumu wa Mulungu patsogolo . Ngakhale zinali conco , Yesu anagwila dzanja la wakufayo , na kukamba kuti : “ Mtsikana iwe , dzuka ! ” ( a ) M’fanizo la Yesu la wofesa mbewu , kodi mbewu na nthaka ziimila ciani ? Anthu ambili amatelo , ngakhale amene sakhulupilila Mulungu . Kuwonjezela apo , analimbikitsa ena kutamanda Mulungu pamodzi naye . — Ŵelengani Salimo 147 : 1 , 7 , 12 . Ganizilani Mose amene anaikidwa kukhala mtsogoleli wa Aisiraeli . Ndipo ophunzila ake anali kuonedwa kuti ndi “ osaphunzila ndiponso anthu wamba . ” Felisa : Nditabatizidwa mu 1973 , ku Santander , likulu la cigawo ca Cantabria , kunali Mboni za Yehova pafupifupi 70 . Ngati amayi ake a Nowa na abululu ake anali moyo pamene Cigumula cinayamba , ndiye kuti anawonongedwa . Koma imwe musasoceletsedwe na njila yake yacinyengo imeneyi . Kunena zoona , vuto limene linabuka pakati pa Eodiya na Suntuke liyenela kuti linasokoneza mtendele wa mpingo wonse . Colinga ca kampeni imeneyi cinali kulalikila anthu ambili m’kanthawi kocepa . 6 / 1 ‘ Tamvelani Maloto Awa ’ ( Yosefe ) , — September - October Yehova anali kuthandiza amuna amenewo poseŵenzetsa angelo . Munthu amene poyamba sanalabadile coonadi , m’kupita kwa nthawi angalabadile cifukwa ca kusintha kwa zinthu mu umoyo wake Ciwombankhanga cimatha kuuluka mtunda utali popanda kukupiza mapiko . Koma sicicita izi mwa mphamvu zake cabe . Pamene tikuyesetsa kulimbitsa uzimu wathu , mzimu woyela udzatithandiza kusanduliza maganizo athu . Kodi nafenso nthawi zina timalephela kuganiza bwino mwa kucita zinthu zimene zingadzutse cilakolako coipa ? Sembe palibe malangizo odalilika otithandiza pa umoyo wathu . 43 : 32 ; 46 : 34 ; Eks . 1 : 11 - 14 ) Ngakhale kuti Aisraeli anali kuvutitsidwa pamene anali kudziko lacilendo , Yehova anawauza kuti aziona mlendo wokhala pakati pawo “ ngati mbadwa . ” — Lev . Mwakutelo , anasonyeza kuti anali wacifundo . — Maliko 5 : 25 - 34 . Conco pamene tikuyembekezela mapeto a dziko loipali tiyeni tiyesetse kukhala ndi makhalidwe abwino . Cifukwa cakuti ngati munthu satsogoleledwa na Yehova pa umoyo wake , ndiye kuti akulamulidwa na Satana . Baibulo lili ndi nkhani zocepa za anthu okhulupilika amene analankhula ndi Yesu pambuyo poti wabwelela kumwamba , ndipo nthawi zina io analankhula ndi angelo . Ganizilaninso za mgwilizano umene timakhala nao padziko lonse poitanila anthu ku msonkhano wacigawo . Sitidziŵa amene analemba salimo limeneli , koma cioneka kuti iye anakhalako panthawi imene Yehova anabwezeletsa Aisiraeli ku Yerusalemu kucoka ku ukapolo ku Babulo . Amai a ku Betelehemu analila kwambili cifukwa ca kuphedwa kwa ana ao . Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa , Buku Lachiŵili , masamba 311 mpaka 318 . Mkhristu angayambe kunyada akaona kuti anthu ambili amakonda mapikica ndi zinthu zina zimene iye amaika pa intaneti . Zimene zinacitikila Abrahamu ca m’ma 1893 B.C.E , zinasonyeza mmene Yehova adzapelekela moyo wosatha kwa anthu omvela . 15 : 1 ; 1 Pet . Nitamva zimenezo , n’nakhumudwa koma sininamuuze mmene n’nali kumvelela . Conco , ise tonse atatu tinaona kuti cikumbumtima cathu cingatilole kusamalila nkhosa m’malo momenya nawo nkhondo ya paciweni - weni . Nkhani iyi idzafotokoza cifukwa cake tiyenela kuimba mokweza na mosangalala , ndipo idzafotokozanso zina zimene tingacite kuti mau athu azicoka bwino poimba . 32 : 4 ) Koma ife ndife opanda ungwilo . Khalani ndi cizoloŵezi coŵelenga nkhani yonse yolembedwa m’caputalaco m’malo mongoŵelenga mavesi oŵelengeka . Iye anali wodzipeleka ndi mtima wonse kwa Yehova cakuti “ anapitiliza kusunga malamulo amene Yehova analamula Mose . ” — 2 Maf . Abale acinyamata ndi acikulile akusangalala kugwila nao nchito yapadela yomanga imeneyi . Iye ‘ anawakwiila kwambili ’ ansembewo , ndipo zimenezi zinaonetsa kuti anali wodzikuza kwambili . Koma zocita zawo zingasokoneze ena amene akuyesetsa kukhala na khalidwe labwino pakati pa anthu a Yehova . — Ŵelengani 1 Petulo 2 : 11 , 12 . Paulo anatilimbikitsa kupemphela kwa Yehova nthawi iliyonse imene tifuna , “ kuti aticitile cifundo ndi kutisonyeza kukoma mtima kwakukulu pa nthawi imene tikufunika thandizo . ” Ndiye cifukwa cake naine sinidzamusiya . Kucita izi kungam’thandize kuona kuti kusamvela kumabweletsa mavuto . Mwacionekele , Adamu anali kudziŵa kale cabwino ndi coipa , cifukwa analengedwa m’cifanizilo ca Mulungu ndipo anali ndi cikumbumtima cabwino . Cina , kuŵelenga Mau a Mulungu kungakuthandizeni kulimbana ndi nkhawa . — Mateyu 11 : 28 - 30 . Anthu ena angakupatseni mankhwala osadziŵika bwino kapena okhudzana ndi zamizimu . ( Mateyu 6 : 31 , 32 ) Komabe , iye amatiyembekezela kucita mbali yathu mwa kugwila nchito mwakhama kuti tipeze zosowa zathu . — 2 Atesalonika 3 : 10 . ( 2 Timoteyo 3 : 15 ) Mofanana ndi amai ake ndi agogo ake , iye anaona kuti Paulo ndi Baranaba anali kukamba zoona zokhudza Mesiya . Onani nkhani imene ili mu Nsanja ya Olonda ya May 1 , 2008 , ya mutu wakuti : “ Kodi Mungadziŵe Bwanji Baibulo Lomasulilidwa Bwino ? Iye sanaleke cizoloŵezi cake copemphela kwa Yehova katatu pa tsiku . Tili ndi ciyembekezo cokondweletsa cotani ca mtsogolo ? Kupemphela kumatiyandikilitsa kwa Mulungu , “ Wakumva pemphelo . ” “ [ Yehova ] anakuitanani kucoka mu mdima kuloŵa m’kuwala kwake kodabwitsa . ” — 1 PET . Onani kuti Yesu anayelekezela Atate ake , Yehova , na mlimi wa mpesa . Kuonjezela apo , Ayuda amene anali kukhala ku Iguputo anali atamasulila Malemba Aciheberi kupita m’Cigiliki . Kodi atumiki a Yehova anaonetsa bwanji kuti amakonda anzao pa ngozi yacilengedwe imene inacitika posacedwa ? Ndi ziyeso zotani zimene acinyamata acikristu amakumana nazo ? N’cifukwa ciani n’kupanda nzelu kugonja ku ziyeso zimenezo ? Nanga tingadziŵe bwanji kuti tayamba kudzikuza ? Mtumwi Yohane anakambapo mfundo yofanana ndi imeneyi . Masiku ano , zofalitsa zathu zikupezeka m’zinenelo zoposa 700 . M’maŵa mwake pamene iye anali kufuna kutulutsa motokayo m’galaji , m’mishonale wina dzina lake Mildred Willett , ( amene pambuyo pake anakhala mkazi wa John Barr ) , anafika . ( Mateyu 24 : 45 - 47 ) Cakudya cimeneci cikuphatikizapo malangizo ofunika kwambili amene anthu a Mulungu amalandila zinthu zikasintha . Nchito iliyonse imene timagwila pa Beteli ni yofunika cifukwa imathandiza “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” kupeleka cakudya ca kuuzimu ku gulu lonse la abale . ( Mat . ( Machitidwe 4 : 18 ) Iwo anapemphela kuti athandizidwe , koma kodi anapemphela kwa ndani ? Ziyeso zimenezo zingaphatikizepo mavuto a m’banja , a ku nchito , kapena matenda . 6 Kodi Baibo Inganithandize Bwanji mu Umoyo Wanga ? Palinso cifukwa cina cimene cipangitsa Yehova kukhala woyenela kulamulila . Ponena za ciphunzitso ca Karma , ndi bwino kudziŵa zimene Baibulo limakamba zokhudza imfa . Tikafunsa funso , tiyenela kumvetsela mosamalitsa yankho la mwininyumba ndi kuona mmene zikum’khudzila . 37 : 25 ; Mat . Kuganizila lonjezo la pa Machitidwe 24 : 15 kumam’tonthoza . Lembali limakamba kuti : “ Kudzakhala kuuka kwa olungama ndi osalungama omwe . ” Cifukwa sanadzidalile . Izi zitanthauza kuti munalonjeza Mfumu ya cilengedwe conse kuti mudzapitiliza kum’tumikila olo kuti anzanu kapena makolo anu aleka kum’tumikila . Mwina inu munaonapo zimenezi . Koma cifukwa comvela cifundo anthu amene anali kumuyembekezela , anayamba “ kuwaphunzitsa zinthu zambili . ” — Maliko 6 : 30 , 31 , 34 . Capakati pa zaka za m’ma 200 B.C.E . , mabuku asanu oyambilila a m’Baibo anamasulilidwa kucoka m’Ciheberi kupita m’Cigiriki . 21 Mmene Masomphenya a Zekariya Amakukhudzilani Malinga n’zimene Baibo imakamba , n’ciani cidzacitikila mabungwe amene anthu ambili amaona kuti ni odalilika ? Wailesi inali kugwilitsidwanso nchito polalikila uthenga wabwino . Mwacitsanzo , Mariya mlongo wa Marita , analinso bwenzi la pamtima la Yesu . Tili na umoyo wosalila zambili . Mtundu wina wa masautso amene tingakumane nao ndi kuukila mwakabisila . Nthawi zina mungakhumudwe cifukwa cakuti mnzanu kapena wina wa m’banja lanu wakulankhulani mau oipa . ( Chiv . 7 : 14 ) Mwacitsanzo , kodi mukuyembekezela kuti m’dziko lililonse mudzakhala nkhondo , munthu aliyense adzasoŵelatu cakudya , ndipo panyumba iliyonse padzakhala wodwala ? Ngati tikucezeledwa na oyang’anila dela , abale ocokela ku mipingo ina kudzakamba nkhani , kapena oimila ofesi ya nthambi , timakhala na mwayi wowaceleza . Komabe , patapita zaka anayamba kutilemekeza cifukwa ca zikhulupililo zathu ndiponso cifukwa ca mmene tinali kulelela ana athu . NYIMBO : 102 , 75 Koma onse aŵili afunika kufika poti aikonzekela nkhaniyo m’maganizo ndi mumtima . Tikafika pa malo okwela , mnzanga wa mu ulaliki anali kundikankha , koma tikafika pamalo otsika ndinali kum’kwezeka panjingayo . Tidziŵa kuti amene anacititsa zimenezi ni Satana Mdyelekezi . Iye ananeneza Yobu kuti anali kulambila Mulungu cifukwa ca dyela . Mfumu Davide anati : “ Ndikakumbukila inu ndili pabedi langa , pa nthawi za ulonda wa usiku ndimasinkhasinkha za inu . ” Cioneka kuti Arimateya ni malo amodzi - modzi amene anali kuchedwa Rama , dela limene masiku ano amati Rentis ( Rantis ) . Mwina nthawi zina cifukwa coopa zimene anthu ena angaganize ndi kukamba , mumalephela kucita zoyenela . Inali nthawi yoyamba kuonako Sinoo ( snow ) . Yosimbidwa ndi Joseph Ehrenbogen Mwamuna ameneyo anali wodzipeleka kwambili ku miyambo ya Ciyuda . Koma pambuyo pake , anaphunzila coonadi . JW.ORG — Pa webusaiti imeneyi pali zida zambili zophunzilila , kuphatikizapo nkhani za pa cigawo cakuti “ Kuyankha Mafunso a m’Baibulo . ” ( Ŵelengani Yohane 15 : 18 - 21 ; Yesaya 2 : 4 . ) Yehova adzapatsa atumiki ake onse mphoto , amene akuimilidwa ndi “ Myuda ” ndiponso amene akuimilidwa ndi “ amuna 10 . ” Iye amafuna kuti tonse tizimvela malamulo ake ndi kukhalabe okhulupilika . Donald wa zaka 19 ku Togo anati , kusintha - sintha “ kwacititsa kuti nkhani zizimveka zatsopano ndiponso kwasintha umoyo wathu wabanja . ” Pankhani yoyamba imene inali kudzakambidwa mu mzinda wa Osaka , abale anaika zikwangwani m’madela onse a mzinda kuti aitanile anthu . Anatumiza tumapepala toitanila anthu tokwanila 3,000 kwa anthu olemekezeka . Sindidziŵa . Onani zimene zinacitika pamene anamwali opusa anapita kukagula mafuta a m’nyali . Mwacionekele , iye anamva cisoni poona zoipa zimene anthu anali kucitila Yosefe , bwenzi lake lolungama . ZOTSATILAPO ZAKE : Ngakhale kuti pali mipukutu yambili ya Baibulo ndipo ina ni yakale kwambili , uthenga wa m’Baibulo sunasinthe . Kukhala pa ubwenzi na Yehova Mulungu kunapulumutsa moyo wanga . Inu mumadziŵa bwino kugwilitsila nchito mfundo za m’Baibo paumoyo wanu . Ndiyeno , tinacoka m’nyumba yathu yaikulu imene tinamanga zaka zaposacedwapa , ndi kusamukila m’kanyumba kakang’ono . Masiku ano , anthu ambili oŵelenga Baibulo ndi okondwa kukhala ndi Baibulo lokhala ndi macaputa ndi mavesi . Izi zimawathandiza kupeza mosavuta uthenga umene afuna , monga mau amene Paulo anagwila m’mipukutu . Baibulo limati : ‘ Mulungu ali kumwamba . Ciliconse cimene afuna kucita amacita . ’ Kumeneko , n’nayamba kutumikila na m’bale Henry Finch na Harry Forrest , amishonale amene anali atangofika kumene kucokela ku Sukulu ya Giliyadi . ( Miy . 6 : 16 , 17 ) Popeza kuti Mulungu ni wacilungamo ndiponso woyela , sanalekelele anthu opha anzawo , olo kuti acita zimenezo mwangozi . Satana amafuna kulepheletsa nchito yomasulila Baibulo , koma tikudziŵa kuti Yehova afuna kuti anthu ake onse azimvetsela kwa iye pamene akukamba nao m’cinenelo comveka bwino . Monga makolo , mungabyale na kuthilila . Ndinaona kuti ndi mwai waukulu kwambili umenewo . Iye anati : “ Ndinasangalala kupatsidwa mwai umenewu . Abale ndi alongo ogontha amagwilitsila nchito cinenelo camanja kutamanda Mulungu . Kodi nthawi zina mumaona kuti moyo ndi waufupi ? Ngakhale pamene akumana na mavuto , aliyense amakhala na maganizo akuti , “ tidzacita ciani ” osati “ nidzacita ciani . ” 20 , 21 . ( a ) Kodi Davide anamutsimikizila za ciani Solomo ? Yobu anati : “ Ngakhale mtengo umakhala ndi ciyembekezo . Iye anacitilidwa zinthu zambili zopanda cilungamo . Tikupemphani kuti muŵelenge maumboni a m’Malemba amene ali pa bokosi oonetsa kuti tikukhala ‘ m’masiku otsiliza . ’ Coyamba , Yehova anapatsa anthu ufulu wodzisankhila zocita . Timawasunga makalata amenewa . 4 : 4 - 7 . ( Yes . 60 : 22 ) Panthawi ina , otsalila odzozedwa anali “ wamng’ono ” koma ciŵelengelo cinakula pamene Aisiraeli ena a kuuzimu anawabweletsa m’gulu la Mulungu . ( Agal . Kodi pophunzitsa ana anu , colinga canu cacikulu ciyenela kukhala ciani ? Kodi mau a Msulami kwa atsikana amene anali kukhala m’nyumba yacifumu ya Solomo amatiphunzitsa ciani ? Kodi iye anati bwanji ? Nthawi zonse , Yesu anali kumvela Atate wake na mtima wonse , olo pamene kucita izi kunali kovuta . Tingapange zosankha zathu komanso kulemekeza ufulu wa ena ( Onani palagilafu 15 ) Iye anatilimbikitsa ngako na mau ake acikondi na okoma mtima . Iwo afika poona Baibo monga coumba cija cimene cafotokozedwa kuciyambi . Sitikukaikila kuti tikukhaladi m’nthawi ya “ mapeto a nthawi ino . ” Ndipo Yehova anaika kale nthawi imene adzaononga dziko loipali la Satana . Akatelo adzakhala ndi cifukwa cosangalalila ndi nchito yake , osati modziyelekezela ndi munthu wina . ” — Agalatiya 6 : 4 . 43 : 10 - 12 ) Kuyambila mu 1938 , kuika paudindo anthu mumpingo mwa kucita voti kunatha , ndipo anayamba kuikidwa paudindo motsatila mfundo za m’Malemba . Tidzaphunzila mfundo zothandiza za mmene tingagwilitsile nchito Baibulo ndi tumapepala twauthenga kuti tiyambitse makambilano , ndi mmene tingafikile anthu pamtima ndi Mau a moyo a Yehova . M’bale wina wa kum’mwela kwa Africa , nayenso poyamba anali kuona kuti kucita zaciwawa kulibe vuto . Komabe , mofanana ndi Hezekiya , aliyense wa ife angauze Yehova m’pemphelo kuti : “ Ndinayenda pamaso panu mokhulupilika ndiponso ndi mtima wathunthu . ” Zimakhala zosavuta ana kulandila cilango na kugwililapo nchito ngati adziŵa kuti makolo awo acita zimenezo cifukwa coŵakonda . 10 : 12 , 13 ) Si zokhazo , Yesu afunikanso kuyembekezela mpaka kumapeto kwa ulamulilo wake wa zaka 1,000 , kuti adani ake onse akatheletu . ( 1 Akor . Anthu ena amati : “ Kukhala pa nchito yapamwamba n’kumene kumapangitsa munthu kukhala wacimwemwe . ” 37 : 25 . Tifunika kuyesetsa kupezamo mfundo zotithandiza . Mtumiki wa m’fanizo la Yesu anadzipezela mabwenzi na zolinga zadyela . Munthu amakhala ndi cikhulupililo mumtima mwake kuti akhale wolungama , koma ndi pakamwa pake amalengeza poyela cikhulupililo cake kuti apulumuke . ” — Aroma 10 : 9 , 10 . Baibulo limati : “ Khamu la anthulo linadabwa kuona osalankhula akulankhula , olumala akuyenda ndiponso akhungu akuona . ” ( Mat . M’baleyo anati : “ Ndithudi ! N’zocititsa cidwi kuona mmene utumiki wathu kuno watithandizila kulimbitsa ubwenzi wathu na Yehova . N’ciani cingakuthandizeni kuti muzisangalala poŵelenga Baibo ndi kuti mupindule na zimene mumaŵelenga ? ( Yobu 13 : 26 ) Pa nthawi ina , nayenso wamasalimo Davide anamvela conco , ndipo anapempha Yehova kuti : “ Musakumbukile macimo a pa unyamata wanga ndi zolakwa zanga . ” Ena amaona kuti sembe cisanduliko si coona , sembe saciphunzitsa ku sukulu . Wiki ina , tingalembe ciŵelengelo ca maola amene tathela pocita zinthu zauzimu , monga kusonkhana , kulalikila , na kucita phunzilo laumwini ndi la pabanja . Zolinga zikulu - zikulu zotenga nthawi yaitali zingakwanilitsidwe mwa kudziikila zolinga zina zing’ono - zing’ono na kuzikwanilitsa . Bwenzi lake Davide anacita zinthu zimene zinakhumudwitsa Yehova . Koma kodi pali umboni wokwanila wosonyeza kuti mankhwala otelo aliko ? 5 : 14 ) Mkristu wozindikila amapanga zosankha zimene zimalimbitsa ubwenzi wake ndi Yehova . Ngati timaona zimene Mulungu amaticitila , tikhoza kuona dzanja lake . NYIMBO : 133 , 63 N’ciani cimakukhutilitsani kuti Yehova ni wadongosolo kupambana wina aliyense ? Ganizilani citsanzo ca Abulahamu na Sara . Pikica yocita kugoba yoonetsa ngalawa yaikulu yonyamula katundu ( m’zaka 100 zoyambilila ) Magazini ino sisankhila anthu mankhwala . Iye sanali kuyembekezela kukwezedwa pa udindo , titelo kukamba kwake . Nawonso makolo angapite ndi ana awo pamaulendo amenewa ngati mpoyenela . Nthawi zonse , Yehova wakhala akupatsa ena mwai wogwila naye nchito pokwanilitsa colinga cake . Masiku ano , ku zisumbu zambili zimene tinapitako , kumapita anthu ambili oona malo . Koma panthawiyo anali cabe malo okhala ndi madzi , micenga , komanso mitengo ya kanjeza . ( Dan . Cimeneci ndi citsanzo cabwino kwambili cofunika kuciganizila makamaka Akristu acinyamata . ( Machitidwe 20 : 28 ) Conco Yehova amafuna kuti akulu azikhala citsanzo cabwino , ndipo io adzayankha mlandu kwa iye cifukwa ca mmene amacitila ndi anthu a mumpingo . Conco , kaya okalamba amenewa ndi acibale athu kapena ai , tiyenela kuwasamalila kwambili . ( Agal . 6 : 10 ; 1 Pet . Ifeyo sitingathe kuonelatu zamtsogolo , koma timafunika kuganizila zotulukapo za zinthu zimene tifuna kucita . ( Mat . 23 : 13 - 36 ) Iye sanagonjele ku zocitika za padziko lapansi . Kaya ndife Akristu obatizika kapena tikufuna kubatizika , tiyenela kuyamikila mwai umene tili nao wogwilizana ndi gulu la padziko lonse la Mboni za Yehova . Inde , cifukwa ca nyengo yabwino , ndipo koposa zonse madalitso a Mulungu , dziko lapansi lidzakhala paladaiso , ndiponso mudzakhala cakudya coculuka . — Salimo 65 : 9 - 13 . Kodi mumasankha kukhala ku mbali ya Yehova mwa kumvela malamulo ndi mfundo zake m’malo mocita zinthu mmene mukufunila ? Iye anamwalila caka catha , ndipo panthawiyo anali m’kagulu ka mpingo wa cinenelo camanja mu Laval , Quebec . Njila imodzi yothetsela mavutowo imachedwa citukuko cosaononga cilengedwe . Zimenezi zikutanthauza kulimbikitsa anthu kugwilitsila nchito zinthu zacilengedwe kutukula cuma ndi khalidwe lao . “ Khamu lalikulu ” la anthu osaŵelengeka , ocokela m’mitundu yonse adzapulumuka pa Aramagedo Angelo ndi zolengedwa zauzimu ‘ zamphamvu . ’ ( Sal . ( 1 Yohane 5 : 14 ) Conco , kuti mapemphelo athu aziyankhidwa , tifunika kudziŵa Mulungu wochulidwa m’Baibulo ndi cifunilo cake . Conco , iye anapatsiwa cilango ca imfa . Kupitila mwa Adamu , imfa inafikila ana ake onse , amene ni mtundu wa anthu . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mafunso amenewa na mmene makolo acikhristu angakhalile ndi kaonedwe koyenela ka ubatizo . “ Kuyambila pamene unali wakhanda , wadziŵa malemba oyela amene angathe kukupatsa nzelu zokuthandiza kuti udzapulumuke . ” — 2 TIM . Kuwonjezela apo , mosiyana na anthu odzikonda amene amangofuna kulandila zinthu kwa ena , atumiki a Yehova amapeza cimwemwe mwa kukhala opatsa . — Mac . 20 : 35 . ( Yer . 23 : 5 , 6 ) Posacedwa , Khristu adzatsogolela makamu akumwamba pogonjetsa mitundu ya anthu kuti akweze Ucifumu wa Mulungu ndi kuteteza anthu a Yehova . ( Chiv . “ Yehova Mulungu wathu ndi Yehova mmodzi . ” Conco , m’pomveka kulichula kuti pemphelo lacitsanzo . Kumeneko , anamunamizila kuti anafuna kugwilila mkazi wa mbuye wake , zimene zinapangitsa kuti amangidwe ndi maunyolo ndi kuikidwa m’ndende . ( Gen . 39 : 11 - 20 ; Sal . Rose akayamba kudzimvela cisoni cifukwa colephela kucita zimene kale anali kucita , amapeza citonthozo pa lemba la 2 Akorinto 8 : 12 , limene limati : “ Mphatso yocokela pansi pa mtima ndi imene Mulungu amakondwela nayo , cifukwa Mulungu amafuna kuti munthu apeleke zimene angathe , osati zimene sangathe . ” N’cifukwa ciani ciwiyaco anapita naco ku Babulo ? Ena amaphunzila mphindi 10 kapena 15 mlungu uliwonse . 1 : 23 - 25 . Tingatengele citsanzo ca Paulo mwa kuvomeleza maganizo olakwika na zikhulupililo zabodza za anthu amene tawafikila , kenako mwaluso tingayambe kuwalalikila “ uthenga wabwino wa zinthu zabwino . ” ( Yes . Kodi muyenela kukumbukila ciani kuti musataye mtima poyembekezela Yehova kuti akuthandizeni kupilila mayeselo ? ( Yobu 7 : 20 ; 13 : 24 ) Mwina tingaganize kuti pamenepa Yobu sanalakwitse cifukwa anali atakumana ndi mavuto ambili . ( Mat . 28 : 20 ) Mmenenso zinthu zinalili padziko panthawiyo ziyenela kuti zinapangitsa kuti nchito yolalikila Ufumu iyende bwino . Mwa njila imeneyi , iwo ndi adzukulu athu anali kutengako mbali mokwanila pa zinthu zauzimu . Ena akuvutika ndi matenda a maganizo kapena cifukwa cakuti anthu ena anawacitila nkhanza . ( Gen . 6 : 5 ) Conco Yehova anaganiza zobweletsa cigumula kuti aononge dziko loipalo . Adzakhalanso onyoza ndi aciwembu , kapena kuti okamba mau opweteka ndi acipongwe kwa anthu anzawo , ngakhale kwa Mulungu . Baibulo limanena kuti ana a Eliyabu , Datani ndi Abiramu , anagwilizana ndi Kora monga atsogoleli kuti aukile Mose ndi Aroni . ( Num . 31 Za m’Nkhokwe Yathu Ndipo timayamikilanso Mulungu kaamba ka “ cakudya calelo . ” YOSEFE WA KU ARIMATEYA anali kuona kuti sangakwanitse kukaonana ndi Pontiyo Pilato , bwanamkubwa waciroma . Koma posacedwa , Satana adzawonongedwa . Cizindikilo ca masiku otsiliza cidzakhala nkhondo , njala , zivomezi , na kuwanda kwa matenda akupha . — Mateyu 24 : 3 , 7 ; Luka 21 : 11 . 77 : 12 , 13 ) Mukamacita zimenezi , ubwenzi wanu ndi Yehova umalimba kwambili . Munthu akaloŵa m’banja , amatetezeka ku macitidwe monga kudzipukusa ( masturbation ) , kapenanso ciwelewele cifukwa cothenthedwa ndi cilakolako . Komanso , n’cinthu canzelu kuganizilanso msinkhu . N’ciani cina cimene cimaonetsa kuti munthu ni wakuthupi ? Iwo amadzipeleka potumikila Yehova na kuika maganizo awo onse pokwanilitsa zolinga zauzimu . Masiku ano , Yehova sangatiuze mwacindunji kuti tilimbikitse munthu winawake monga mmene anauzila Mose kulimbikitsa Yoswa . Susan ndi mlongo wolimba ndiponso wauzimu . Kodi si paja Yesu anasandutsapo madzi kukhala vinyo ! ( Ŵelengani Machitidwe 13 : 34 . ) Kuwonjezela pa madalitso auzimu amene akusangalala nawo tsopano , atumiki a Yehova Mulungu okhulupilika akuyembekezela mwacidwi kudzalandila madalitso aakulu m’tsogolo . 2 : 13 - 17 . Kodi atumiki akale a Yehova anapeleka citsanzo cotani pankhani yomvela ndi kulemekeza boma ndi olamulila ? Ambili aife tinganene kuti inde . 11 : 4 ) Zimenezi zitikumbutsa zoikapo nyale ndi mitengo iŵili ya maolivi , yochulidwa mu ulosi wa Zekariya . Nthawi zina tinali kulumiwa na tudoyo . Mulungu anayankha mapemphelo a anthu amene anapemphela ali ‘ cokhala pansi , ’ ‘ coimilila , ’ ‘ cogona ’ kapena ‘ cogwada . ’ Kodi makolo ena athandiza bwanji ana awo kukhala na zolinga zauzimu ? Nanga apeza mapindu anji cifukwa cocita zimenezi ? 12 , 13 . ( a ) Pelekani citsanzo coonetsa mmene umbombo ungatitsogolele ku ngozi . ( b ) Fotokozani mmene umbombo ungakulile mofulumila ngati siticitapo kanthu . Koma aliyense aziganiza m’njila yakuti akhale munthu woganiza bwino , malinga ndi cikhulupililo cimene Mulungu wamupatsa . Anthu omvela adzaonetsa cikondi kwamuyaya . PITILIZANI KUKONDA ANZANU MMENE MUMADZIKONDELA Kale , Atate wathu wacikondi wakumwamba anathandiza atumiki ake . Ndipo masiku anonso , amatithandiza kucepetsa nkhawa kapena kuvutika maganizo . Na ise tingatengele Paulo na Sila mwa kuganizila zotulukapo zabwino zimene zimakhalapo cifukwa cotumikila Mulungu mokhulupilika . — Afil . M’maiko ambili , n’zosadabwitsa kumvela anthu akukamba kuti sakhulupilila kuti kuli Mulungu . Amadziona kuti ni anthu osapembedza . Mungaonenso mbili ya moyo wa Hadyn ndi Melody Sanderson pa mutu wakuti “ Kudziŵa ndi Kuchita Chabwino , ” mu Nsanja ya Olonda ya March 1 , 2006 . Pitilizani kucita kulambila kwa pabanja na phunzilo laumwini nthawi zonse . Yesu anakamba mfundo yosavuta imene ingatiteteze ku mabodza a Satana . Kodi Aisiraeli anacita ciani atapemphedwa kupeleka zopeleka ? Ndipo mavuto ambili amene anthu akukumana nawo masiku ano amabwela cifukwa ca kusadziletsa . ( 2 Akorinto 12 : 7 , 8 ) Mwina Paulo anali ndi vuto lalikulu la maso . Mau awa ndi olimbikitsadi cakuti tingakambe kuti : “ Yehova ndiye mthandizi wanga . 6 : 1 - 3 ) Koma bwanji ngati mnzanu wa m’cikwati satsatila mfundo za m’Baibo za makhalidwe abwino ? Umphawi : Malinga ni lipoti ya World Bank , ciŵelengelo ca anthu osauka kwambili mu Africa mokha cinawonjezeka kucoka pa 280 miliyoni mu 1990 , kufika pa 330 miliyoni mu 2012 . Pa tsiku limene Samueli anakumana ndi Sauli , mneneliyu akanangodzoza Sauli popanda kumukonzekeletsa . Iye akanangotenga botolo la mafuta ndi kuthila pa mutu pa Sauli mwamsanga ndi kuuza mfumu yatsopanoyo kuti izipita . Cuma cambili ca Aiguputo cimene anakana cinafunkhidwa ndi Aisiraeli . ( Eks . Conco , m’kalata yake yoyamba yopita kwa Akhristu aciyuda ndi a mitundu ina amene anali kukhala ku Asia Minor , Petulo anafotokoza za kufunika kokonda gulu lonse la abale . — 1 Pet . Mulungu Wamphamvuyonse ali ndi mphamvu yocita zimenezo ndipo amafunitsitsa kutelo . 6 : 1 ) Yehova amatisamalila mwacikondi kudzela mwa “ mphatso za amuna . ” ( Aef . 18 : 11 , 12 ) Mfumu Davide atakalamba “ sankamva kutentha . ” ( 1 Maf . M’kupita kwa nthawi , abale ndi alongo a mumpingo wa Oswestry anakhala ngati banja lathu latsopano cifukwa anali kutithandiza pa mavuto athu mwacikondi . Komabe , zida zonsezi zatithandiza kunola luso lathu pa nchito yolalikila . Fotokozani citsanzo coonetsa mmene mabwenzi eni - eni amatonthozela ngati acibale athu alephela kucita zimenezo . Milan anangokhala cete cifukwa ca mantha . Komabe , anthu a Yehova aonetsa khama pofuna kupeza anthu acidwi kumadela akutali m’dzikolo . Kutengela citsanzo cawo kudzatithandiza kumakonda anthu ena na kuwalimbikitsa pa nyumba yathu na ku Nyumba ya Ufumu . Rogelio anati : “ Zinali zovuta kwambili kusiya mabanja ndi mabwenzi athu . ” Komabe tisaiwale kuti Satana angagwilitsile nchito dzikoli kuti atisonkhezele kucita chimo kapena kuyamba kukonda zinthu za m’dzikoli ndi kusiya kulambila Yehova . — Ŵelengani 1 Yohane 2 : 15 , 16 . ( Luka 4 : 18 ) Kodi izi zinatanthauza kumasuka mu ukapolo weni - weni ? Iye amatifotokozela zimene tiyenela kucita kuti tizigwila nchito mogwilizana ndiponso mwamtendele ndi anthu onse a m’banja lake . Baibulo la Dziko Latsopano limene linakonzedwa mu 1984 linafotokoza kuti Yehova angathe kukhala ciliconse cimene angafune kuti akwanilitse zimene analonjeza . Kodi Yehova anathandiza bwanji anthu amene anacita zinthu mogwilizana panthawi imene Aisiraeli anali kucoka mu Iguputo ? ( Ŵelengani Salimo 37 : 29 . ) ▪ Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo — Mbali 1 Akhoza kusintha nthawi iliyonse . Koma ine n’nangoloŵa m’cipinda canga na kukhoma citseko . ( Aheb . 11 : 10 ) Iye “ anakhulupilila mwa Yehova , ndipo anaonedwa ngati wolungama . ” — Aroma 4 : 3 . Mu 36 C.E . , Mulungu anagwilitsilanso nchito Petulo kupeleka mwai kwa ena kuti akhale mtundu watsopano wa Isiraeli wa kuuzimu . Conco , Yesu ayenela kuti anali kufuna kudziŵa cimene Petulo anali kukonda kwambili . Kusintha kumeneku n’kofunika ngako . Baibo imayelekezela mtundu wa anthu na nyanja imene ikuwinduka , imene ikulephela kukhala bata . ( Yes . 17 : 12 ; 57 : 20 , 21 ; Chiv . Patapita nthawi yocepa , iye analowa m’nyumba yacifumu yolemekezeka ndi kuimilila pamaso pa Farao . Mwacitsanzo , mungakhale ndi colinga cokulitsa cipatso ca mzimu cimene muona kuti cimakuvutani kukulitsa . Patapita masiku atatu , zimene Yosefe anakamba zinacitikadi . N’cifukwa Ciani Yesu Anavutika ndi Kutifela ? Iwo adzasangalala kukambilana nanu nkhaniyi . [ Mau apansi ] Dipo ni malipilo a cinthu cimene cawonongeka , kapena malipilo olipilidwa kuti munthu amasuke m’ndende . Ngati timamvela amene akutitsogolela mwa kukhala okhutila ndi osangalala ndi utumiki uliwonse umene tapatsidwa ndiye kuti m’dziko latsopano tidzaonetsanso khalidwe limenelo . KODI kukhala mboni kumatanthauza ciani ? N’cifukwa ciani tiyenela kupeleka lipoti lathu la mu ulaliki ? MBILI YANGA : NDINALI KUKONDA MANKHWALA OSOKONEZA UBONGO NDIPO SINDINALI KULEMEKEZA AKAZI Malemba amalangiza amuna kuti : “ Musaleke kukonda akazi anu ndipo musamawapsele mtima kwambili . ” Koma patapita zaka 400 , anthu anali atatalikilana kwambili na ungwilo . Pamsonkhano wina mu 1950 m’dziko la United States , mlongo Annie Poggensee anapindula kwambili pamene anaimilila pa mzele kwa nthawi yaitali ngakhale kuti kunali kotentha . Tsopano Rabeka anafunika kupanga cosankha cacikulu pamoyo wake . Zakhala zakuti coonadi conena za Mulungu caphimbidwilatu . M’malo mwake , anati : “ Tiyenela kukumana ndi masautso ambili kuti tikaloŵe mu ufumu wa Mulungu . ” Masiku ano , anthu mamiliyoni amakamba kuti anthu amavutika cifukwa ca ciphunzitso ca Karma , kapena kuti zimene munthu anacita m’moyo wina asanabadwenso . Analukamba za nkhani imene anthu angakambilane ndi kuithetsa pakati pawo kumbali . Yehova anasankha Elisa kuti adzalowe m’malo mwa Eliya . “ ANZANGA atanifotokozela zocitika zosangalatsa zimene anakumana nazo potumikila ku madela amene kunali apainiya ocepa , n’nayamba kulaka - laka kuti nikalaŵeko utumikiwo , ” anatelo Sylviana , mpainiya wa zaka za m’ma 20 . Mwamsanga Akristu onse okhulupilika a mumzindawo ndi a m’madela ozungulila anathaŵila ku mapili a ku mtsinje wa Yorodano . Iye anaonetsapo cikondi cimeneci akali kumwamba ndiponso atabwela padziko lapansi . ( 1 Yoh . 2 : 1 , 2 ) Izi ndi zina mwa zinthu zambili zimene tingacite zoonetsa kuti timakonda Yehova cifukwa ca cikondi cake cosatha . Coyamba , anapewelatu tsankho . Tingacite ciani kuti mkwiyo usakatimanitse mphoto ? Iye anati : “ Inu Yehova ndikomeleni mtima , ndicilitseni pakuti ndakucimwilani . ” Anaonjezelanso kuti : “ Cilamulo ca Yehova ndi cangwilo , cimabwezeletsa moyo . ( Mika 5 : 7 ; Yohane 10 : 16 ) Uthenga umene timalalikila ndi njila ina imene Yehova amathandizila anthu amene ali ndi ludzu la coonadi kuti adzapeze moyo . Kodi Mfumu inalimbikitsa motani atumiki ake a padziko lapansi kuyamba kulalikila ? 1 : 6 ) Conco inu makolo , musaleme polangiza ana anu , koma pitilizani kuwaphunzitsa moleza mtima . ( Aef . 20 : 13 * M’kati mwa ulendowo , tinacita ngozi mu Texas cakuti motoka yanga inawonongekelatu . Kuyambila nthawi imeneyo , io sanavutitsidwenso pa nkhani imeneyi . N’cifukwa ciani anthu ambili analephela kumvetsetsa tanthauzo la mau a Yesu ? Nayenso munthu amene wacotsedwa mumpingo wacikristu , umene ndi banja lake lakuuzimu , angazindikile kuti anataya mwai . 18 : 22 ) Ngakhale n’conco , Malemba amakambilatu kuti anthu opanda ungwilo akamanga banja , “ adzakhala ndi nsautso m’thupi mwawo . ” ( 1 Akor . Mu alifabeti ya Cigiriki , kacilembo kocepetsetsa ni iota . Mwacionekele kacilembo aka kalinganako na kaciheberi י ( yod ) . Ufumu umenewu unali wokondwa kukhala na mtendele woculuka komanso cuma . Ena amene anali kumwa moŵa kwambili asanakhale Mboni , anasankha kulekelatu kumwa moŵa . Mlongo winanso dzina lake Brigitte , amene analela yekha ana aŵili pambuyo pakuti mwamuna wake wamwalila anati : “ Kulela ana m’dziko la Satanali n’cimodzi mwa zinthu zovuta kwambili makamaka ngati ukuwalela wekha . Kodi anthu anakhala bwanji mbali ya banja la Mulungu ? Khama lawo pa nchito yolalikila linawonjezeka . Conco , m’masiku otsiliza ano , tiyeni tonse tikhale oyela m’makhalidwe athu , ndi kukhala kumbali ya ulamulilo wa Mulungu wathu woyela , Yehova . Tingaonetse bwanji kuti timam’konda Mulungu ? Mu 1959 , ananimanga cifukwa copulinta mabuku ophunzitsa Baibo . Nkhani ina m’magazini yakuti Biblical Archaeology Review ya mu 2014 , inayankha funso yakuti : “ Ni anthu angati ochulidwa m’Malemba Aciheberi amene umboni wa zinthu zakale watsimikizila kuti analiko ? ” Anafunikilanso kuzoloŵela mipingo yatsopano , kulalikila m’magawo atsopano , mwina ngakhale kulalikila m’cinenelo cina . Anthu ambili amakamba kuti pali Mlengi amene anapanga zamoyo . — Ŵelengani Salimo 139 : 13 - 17 ; Aheberi 3 : 4 . Ambili a io alemba makalata oyamikila cifukwa cokhala ndi Nsanja ya Mlonda imeneyi . 5 : 1 , 5 - 7 , 12 ) Ngati akulu agamula kuti munthu wosalapa acotsedwe mumpingo , ife tiyenela kuciliciza cigamulo cimeneco . 7 : 46 ) Kodi inuyo mumayesetsa kutengela citsanzo cake pa nchito yolalikila mwa kugwilitsila nchito mau ogwila mtima polalikila ? — Akol . Koma ubwenziwu ungasokonezeke cifukwa cakuti tikukhala m’dziko la Satana loipali ndiponso cifukwa ca thupi lathu lopanda ungwilo . Anthu omasulila mabuku opitilila pa 2,900 alandila maphunzilo apadela owathandiza kumasulila Baibulo ndi mabuku ofotokoza Baibulo . 3 : 21 , 22 ; 35 : 22 - 24 ) M’nthawi ya atumwi , Akhristu ena anali kugulitsa zinthu zawo , monga minda na nyumba , ndipo ndalamazo anali kuzipeleka kwa atumwi . Ngakhale kuti Yesu sanali Mlevi , akanaimililabe pa dengalo , ndipo palibe amene akanamuletsa . Nanga , kodi tsogolo lanu lidzakhala bwanji ? Ndipo yesetsani kulemekeza Mulungu m’malo modzifunila ulemelelo . ( Sal . 18 : 37 - 40 ) Eliya anali ndi ciyembekezo cakuti anthu a Mulungu adzayambanso kulambila koona , koma zimenezo sizinacitike . Timakhulupilila kuti Iye aliko ndi kuti salephela kupeleka mphoto kwa amene amawakonda . — Ŵelengani Aheberi 11 : 6 . Akristu oona amakhulupilila zimene Baibulo limanena ndipo amakhalanso moyo mogwilizana ndi zimene limanena . Iye anaphunzila coonadi ndipo anabwelako mu 1956 . N’nakwanitsa ngakhale kulalikila na kugaŵila tumapepa twauthenga mumsewu . Komanso , kudzatipatsa mwayi wolandila cisomo ca Mulungu . ( a ) Malinga n’zimene Zekariya anaona , n’ciani cina cimene cinacitikila ciwiya copimila ? 11 : 13 - 15 ) Cinanso , Satana amafalitsa mabodza poseŵenzetsa anthu oyendetsa zamalonda . Iye anakamba kuti pambuyo popemphela mobweleza - bweleza na kusinkha - sinkha mfundo zolimbikitsa za m’Baibo , anayamba “ kuona mavuto kukhala mwayi osati zopinga . ” 45 : 23 , 24 ) Kodi mufuna kukhala mmodzi wa anthu ocilikiza ulamulilo wa Yehova mokhulupilika ? Koma cifukwa cakuti sititenga mbali m’ndale , ndife ogwilizana ndi abale ndi alongo athu padziko lonse . — 1 Petulo 2 : 17 . Odzozedwa amenewa adzakhala “ olandila coloŵa anzake a Kristu , ” ndipo adzakhala ndi mwai wokhala “ ufumu wa ansembe . ” Sitidziŵa kuti kaya zinthu zidzatiyendela bwino kapena ayi . Ndiye cifukwa cake ngakhale anthu apange zosankha zooneka zabwino , nthawi zina zimawabweletsela mavuto na masoka . ( Miy . Peter anafunsa munthuyo ngati anali kufuna kumvetsetsa Baibo . ( Onani ndime 11 - 16 ) Kukulitsa mzimu wa kudzicepetsa n’kofunika pa zifukwa ziti ? ( Ŵelengani 1 Timoteyo 517 ) Abale amenewa timawalemekeza mosasamala kanthu kuti ndi olemela kapena osauka , ophunzila kapena osaphunzila , kapena kuti acokela ku dziko liti . Paciyambi penipeni , Mulungu anagwilitsila nchito Ciheberi pokamba ndi Adamu , koma Yehova amakamba ndi anthu m’cinenelo ciliconse . Mwacitsanzo , anthu ena anali kudya mkate ndi kumwa vinyo pa Cikumbutso , koma patapita nthawi analeka . CAPAKATI pa 62 na 64 C.E . , mtumwi Petulo analembela kalata ‘ alendo osakhalitsa , amene anali atamwazikana ku Ponto , Galatiya , Kapadokiya , Asia , ndi ku Bituniya . ’ ( 1 Pet . Iye anawauzanso kuti azipeleka mphatso zacifundo ‘ mwamseli ’ kapena kuti mosaonetsela . Kuyambila ca m’ma 1950 , zocita za anthu n’zimene zapangitsa kutentha kumeneku . ” — American Meteorological Society , 2012 . Iye anali kudziŵa zimene zinali m’mitima yao . Ophunzila a Yesu analinso alangizi a Mau a Mulungu . Kuonjezela pa kuŵelenga Baibulo tsiku lililonse , tifunika kuliphunzila pogwilitsila nchito zofalitsa zathu monga Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani . Ngati amacitila nkhanza mkazi wake ndi kum’kakamiza kuti azim’lemekeza , sangaphule kanthu . Kodi sitinayamikile cikondi na kukoma mtima kumene abale na alongo anationetsa mwa kutikhululukila ? ( Yoh . 10 : 16 ) Popeza Mdyelekezi watsala ndi kanthawi kocepa , colinga cake n’cakuti ameze atumiki ambili a Yehova mmene angathele . Pokhala Mboni za Yehova zodzipeleka , timadziŵa zimene zidzacitika mtsogolo , ndipo tili ndi ngongole youzako ena zimene timaphunzila . Tiyeni tikambilane zinthu zitatu zimene mungacite poŵeta ana anu . Muyenela kuwadziŵa bwino , kuwaphunzitsa , ndi kuwatsogolela . N’nalinso kuchova njuga za mitundu yosinaya - siyana . Palinso abale na alongo ena amene pa zifukwa zina analeka kucita utumiki wa nthawi zonse , koma akali kuulaka - laka . Nawonso angayamikile ngati tiwalimbikitsa . Koma iye sanalole kuti nkhawa imeneyi imulepheletse kusankha kutumikila Mulungu . Ngati sanaukitsidwe sitikanamva za iye . Paulo anacha mpando wacifumu wa Yehova kuti “ mpando wacifumu wa kukoma mtima kwakukulu , ” ndipo anatilimbikitsa kuti tiyenela kupemphela kwa iye “ ndi ufulu wa kulankhula . ” Unali ulendo wautali pafupifupi makilomita 800 , ndipo uyenela kuti unatenga milungu itatu . Mwina timaganizila za malo ena m’dziko latsopano amene tingakonde kudzakhalako , koma tingadzapemphedwe kukhala malo ena . Mabwenzi athu apamtima ayenela kukhala anthu ocita cifunilo ca Mulungu . ( Akolose 2 : 8 ; 1 Yohane 2 : 15 - 17 ) Kodi tingapewe bwanji zimenezi ? Patapita zaka zoposa 800 pambuyo pa Cigumula , Mulungu anapanga Aisiraeli kukhala mtundu . Iwo anaona mmene Yesu anaonetsela kulimba mtima . ( Mat . ( b ) Fotokozani citsanzo coonetsa mmene Yehova amamvelela tikadzipatulila kwa iye . ( 2 Akorinto 3 : 18 ) Tidzapitilizabe kuphunzila zambili zokhudza Atate wathu wakumwamba ndi kumutsanzila kwamuyaya . Pa maulendo ao , a gulu loonetsa seŵelo la “ Eureka , ” anali kugwilitsila nchito ngolo yokokedwa ndi mahosi yonyamulila katundu wao wonse . Kodi Amacita Nanu Cidwi ? — September - October Koma nthawi ya ukapolo inali itapita , ndipo anakhala amisili aluso pamene Yehova anawasankha kuti atsogolele pa nchito yomanga cihema . ( Eks . Nthawi zina tinali kuona ngati palibe amene angatithandize . Timoteyo ayenela kuti anaphunzila Cikhristu m’caka ca 47 C.E . , pa ulendo woyamba wa mtumwi Paulo wokacezela Akhristu a ku Lusitara . Cipilala ca Tito cili na zosema ziŵili zikulu - zikulu zoonetsa cocitika codziŵika bwino cokhudza mbili yakale . Pali ubale wotani pakati pa cilungamo ndi kusamvela malamulo ? Mwacitsanzo , tiyelekeze kuti mwana wakamba mopanda ulemu kwa kholo lake . Mawu olakwikawo anayamba kupezeka ngakhale m’Baibulo yochuka yacingelezi ya King James Version . Citani ciliconse cotheka kuti mupitilize kukhala ocilimika . Kudziŵa kuti abale ndi alongo athu ena ndi ofooka cifukwa ca kudwala , kukhala m’mabanja ogaŵanika , kapena cifukwa covutika maganizo , kungaticititse kukhala ofunitsitsa kuwathandiza . Popeza n’zosatheka munthu mmodzi kulalikila ku “ mitundu yonse , ” ophunzila ake anayenela kukhala gulu locitila zinthu pamodzi . ( Mac . 13 : 50 ; 14 : 2 , 19 ; 18 : 12 , 13 ) Onani cocitika cimodzi ici . Anthu ambili akaganizila kukula kwa cilengedwe conse , amakhala ndi funso lakuti , ‘ N’cifukwa n’ciani Mlengi wamphamvuyonse amayang’anila zocita za anthu otsika amene ali pa kapulaneti kakang’ono ? ’ Kodi anali kudzitama ? Ngati zilidi conco , mosakaikila cikhulupililo colimba ca Sara cinapangitsa kuti aziuzako ena za Mulungu wake ndi ciyembekezo cake mowafika pamtima . Ulosi wa pa Ezekieli 37 : 1 - 14 , umanena za anthu onse a Mulungu amene anayambanso kulambila koona mu 1919 , pambuyo pa zaka zambili za ukapolo . 48 : 1 - 4 , 10 ; Aheb . 11 : 21 ) Mlongo wina wa zaka 93 dzina lake Ines , amene akudwala matenda amene amafooketsa minofu , anati : “ Tsiku lililonse ndimaona kuti Yehova akundidalitsa . Mwacitsanzo , ganizilani zimene Mulungu anacitila Loti . ( Luka 5 : 13 ) Yehova anapatsa Kristu mphamvu yocita zozizwitsa n’colinga cakuti Yesu aonetse kuti amakonda kwambili anthu . — Luka 5 : 17 . Koma anthu m’dziko la Satanali si osangalala ndipo alibe ciyembekezo codalilika . Uzionetsetsa kuti walalikila munthu aliyense asanacoke pabedi . ” 2 : 16 , 17 . Ana ena akakhala pachuthi amapita kukaona makolo ao , kuŵasamalila , ndi kuŵathandiza nchito zimene sangathe kugwila . Abale ena anali kutengelana ku makhoti . Muyenela kukonzekela tsopano zinthu zocititsa cidwi zimenezi mwa ‘ kupitiliza kupilila moleza mtima ngati kuti mukuona Wosaonekayo . ’ Paulo anaonetsa kuti anthu amene ali na udindo wolimbikitsa ena , nawonso amafunikila cilimbikitso . Koma Yohane M’batizi anawauza kuti : “ Mulungu ali ndi mphamvu yokhoza kuutsila Abulahamu ana kucokela ku miyala iyi . ” — Luka 3 : 8 . Anam’limbikitsa kuti aziyamikila maudindo amene anapatsidwa , ndi kuti ayenela kupita patsogolo mwa kuuzimu . Baibo imatilangizanso kuti tiyenela kukhala pa ubwenzi na Mlengi wathu . Cifukwa ca cikhulupililo , Mose sanaike maganizo ake pa zinthu zooneka ndi maso . Kangapo konse , ndeke zopita kwawo sizinapite cifukwa ca zovuta zina . Nyumba yathu itapsa , tinasamukila kwa makolo a mkazi wanga . Cikumbumtima cophunzitsidwa bwino sikuti cimangoticenjeza tikafuna kucita zoipa , koma cimatilimbikitsanso kucita zinthu zabwino . ( 1 Mafumu 21 : 3 ) Kodi Naboti anali wamwano ? Zioneka kuti nchito yomasulila malembawa inayamba zaka pafupifupi 300 Kristu asanabadwe ndipo inatha pambuyo pa zaka 150 . ( 1 Pet . 4 : 7 ) Muziganizila zitsanzo zabwino za abale na alongo amene ali na umoyo wacimwemwe cifukwa cokhalabe maso mwauzimu na kuonetsa kuwala kwawo . 4 : 29 , 31 . Rudy kusankha mau abwino ? Conco ndinapatsidwa udindo wophunzitsa Baibulo mlungu uliwonse pa misonkhano imene inakonzedwela akaidi . Anati : “ Akanakhala kuti anali kumangokumbukila malo amene anacokela , mpata wobwelela akanakhala nawo . ” 12 : 28 ) Mofanana ndi Yesu , ifenso tiyenela kukhutula mtima wathu kwa Mulungu m’pemphelo . ( Sal . Abulahamu anali kum’konda Isimaeli , ndipo monga kholo sanafune kukhala zii . Komabe , Yehova anali kuidziŵa nkhani yonse . Koma cikondi cidzatisonkhezela kucita zimenezo . Ambili amatenga ngongole ndipo mau akuti “ wobweleka amakhala kapolo wa wobweleketsayo , ” akwanilitsidwa pa io . — Miyambo 22 : 7 . Baibulo limati : “ Mkwati anafika , ndipo anamwali okonzekelawo analoŵa naye limodzi m’nyumba imene munali phwando laukwati , ndipo citseko cinatsekedwa . ” ( Yer . 22 : 17 - 19 ) Zedekiya mwana wa Yosiya ndiponso mdzukulu wake Yehoyakini naonso analephela kutengela citsanzo cabwino ca Yosiya . — 2 Maf . Timapempha Yehova kuti atithandize kukhala olimba mwa kuuzimu ndi kuti tikhale acangu pa nchito yolalikila . ” Komabe , simuyenela kudela nkhawa kwambili ndi maonekedwe anu mpaka kufika polephela kucita zinthu “ mwanzelu . ” Apa , iye anali kuwalimbikitsa kuti aziceleza Akhristu anzawo . Mwacitsanzo , Ayuda otsutsa ocokela ku Ikoniyo ndi ku Antiokeya anafika ndi kusonkhezela anthu a mumzindawo kuti aukile Paulo ndi Baranaba . Mungacite bwino kusinkha - sinkha mfundo zothandiza izi . mu Nsanja ya Olonda ya May 1 , 2008 . ( Gen . 3 : 14 - 19 ) Ngati anawapha nthawi imeneyo , cifuno cake ponena za Adamu ndi Hava ndi mbadwa zao cikanathela pamenepo . ( Yes . Paulo analangiza kuti : “ Muikeni cizindikilo ndipo lekani kucitila naye zinthu limodzi . ” Kalata ya Paulo mwacionekele inalimbitsa cikhulupililo ca Timoteyo . Inam’kumbutsa zimene zinacitika pamene Aroni wokhulupilikayo anayanjidwa ndi Mulungu . Inam’kumbutsanso zimene zinacitika pamene cinyengo ca Kora ndi anzake cinadziŵika . * Cidindo pa “ maziko olimba a Mulungu ” cinali ndi mauthenga aŵili . Pitilizani kudziyesa kuti mudziŵe kuti ndinu munthu wotani . ” — 2 Akor . Abale akuwatenga pambuyo poimbidwa mlandu ( Num . 20 : 12 ) Yoswa ananyalanyaza kufunsila malangizo kwa Mulungu asanacite pangano ndi Agibeoni . ( Yos . Komabe , mwina mumakhalako na nkhawa . ( b ) N’cifukwa ciani okwatilana ayenela kuuzana mau acikondi ? NYIMBO : 125 , 62 Caciŵili anayamikila kukoma mtima kumene Boazi anamuonetsa . Ena anali kugona m’nyumba za anzao , ndipo ena anali kugona ku nyumba za alendo . Ngakhale kuti mwatumila munthu mmodzi uthenga winawake , munthuyo angathe kutumila anthu padziko lonse m’masekondi ocepa cabe . Yehova atatsala pang’ono kusamutsila moyo wa Mwana wake m’mimba mwa Mariya , anatumiza mngelo kuti akakambe naye . Tifunika kuyendetsa motoka mosamala , olo kuti tiyenda ku misonkhano . 4 : 5 ) Tiyeni titsanzile mtumwi Paulo amene analemba kuti : “ Ndikucita zinthu zonse cifukwa ca uthenga wabwino , kuti ndiugaŵilenso kwa ena . ” ( 1 Akor . Kuti mupeze yankho , muyenela kuyelekezela zimene chechi yanu imaphunzitsa ndi zimene Baibulo imakamba . Patangopita nthawi yocepa , Antonio anakhala mkulu . 33 : 13 . Nkhani yoyamba pa nkhani ziŵili izi idzafotokoza mmene Yehova anathandizila ophunzila a Yesu m’nthawi ya atumwi kulalikila uthenga wabwino . Olo kuti anacita zimenezi , iye anati : “ N’napitilizabe kudzimvela cisoni . Ndiyeno , n’napemphela kwa Yehova ndi mtima wanga wonse . Fotokozani cifukwa cake sitidzafunikila kucita mantha pa cisautso cacikulu . Ndiyeno , anafotokoza mmene tingakhalile oyela . ( b ) Kodi tidzakambilana ciani m’nkhani yotsatila ? ( Gen . 2 : 9 ) Kukamba zoona , nthawi zambili ise anthu sitidziŵa kuti zosankha zathu zidzakhala na zotulukapo zabwanji . Mwacitsanzo , Mabuku Apacaka a mu 1992 , 1999 , ndi 2008 amafotokoza nkhani zolimbikitsa za abale a ku Ethiopia , Malawi , ndi ku Russia . Ndiponso , popeza kuti cimwemwe ni mkhalidwe wofunika kupitilizabe , uli ngati ulendo , osati kumene ukupita . Yehova amanyansidwa na kuba kwa mtundu uliwonse . Pambuyo pake , analembanso kuti : “ Limbikilani kupemphela . ” ( 1 Ates . Koma cifukwa codalila Yehova , molimba mtima anabisa amuna aŵiliwo ndi kuwathandiza kuti abwelele kwawo bwino - bwino . Ena anaticenjeza kuti tizipewa kugona m’makalavani kuopela kuti otsutsa angatitenthele mmenemo . Anawauza kuti : “ Tiyeni tiganizilane kuti tilimbikitsane pa cikondi ndi nchito zabwino . Kodi tingatsatile motani citsanzo ca Mulungu wathu wacikondi ? amakupatsilani cilango ? 3 “ Zilumba Zambili Zisangalale ” Ngati titengela Yehova pocita zinthu , timaonetsa kuti tikucilikiza ulamulilo wake . — Ŵelengani Aefeso 5 : 1 , 2 . 1 : 27 - 29 ; 2 : 8 , 9 , 15 ) Koma kodi izi zitanthauza kuti Adamu na Hava anali na ufulu wocita ciliconse cimene anali kufuna ? Koma mwamuna wanga anandilimbikitsa mwa kundiuza kuti : ‘ Usavutike ndi zimene anthu amakamba . Koma atalapa , sanakayikile kuti Mulungu anamukhululukila kupitila mu nsembe ya dipo la Yesu . Kodi tonse tingalimbikitse bwanji mgwilizano mumpingo na kuthandiza ena kuonetsa kuwala kwawo ? Mofananamo , ife tikhala m’masiku otsiliza a dzikoli . ( Luka 14 : 12 - 14 ) Komanso bwanji ngati Mkhristu mnzathu wagwa m’mavuto azacuma cifukwa cosayendetsa bwino zinthu kapena ngati sanayamikile pa zabwino zimene tinamucitila ? ( Mateyu 7 : 15 ) Nayenso mtumwi Paulo anacenjeza Akristu a ku Tesalonika kuti : “ Wina asakunyengeni pa nkhani imeneyi m’njila iliyonse . Pakuti tsikulo [ tsiku la Yehova ] silidzayamba kufika mpatuko usanacitike , ndiponso asanaonekele munthu wosamvela malamulo , amene ndiye mwana wa cionongeko . ” — 2 Atesalonika 2 : 3 . Mwacitsanzo , Mfumu Ahaziya , mwana wa Ahabu ndi Yezebeli , anali kufuna kudziŵa ngati cilonda cake cidzapola . Mungacite daunilodi Baibo imeneyi pa webusaiti ya jw.org kapena mungacite daunilodi JW Library . Baibulo la Dziko Latsopano Lomasulira Malemba Achigiriki Achikhristu linasindikizidwa mu Cidachi , Cifulenci , Cijelemani , Citaliyana , Cipwitikizi , ndi Cisipanishi . 27 : 57 ) Mwacionekele , Yosefe anakopeka na uthenga wa Yesu cifukwa cakuti anali kukonda coonadi ndi cilungamo . Ndikhulupilila kuti sitinakambilanepo nkhaniyi . Mwacitsanzo , amishonale ambili otsiliza maphunzilo a Giliyadi akatumiziwa ku dziko lina , amakhala kumeneko zaka zambili asanabwelele ku dziko lawo kukaceza . Koma timadziŵanso kuti pemphelo lakuti : “ Ufumu wanu ubwele . * Koma n’zosatheka kuti akulu azilengeza zimenezi nthawi zonse . Ni mfundo yofunika iti imene tiphunzilapo pa citsanzo ca Ida ? Nanga tingapeleke bwanji cilimbikitso cogwila mtima ? Onsewa amadzimana zinthu zina mu umoyo wawo kuti azithela nthawi yambili pocita utumiki wopatulika . Iye anakamba kuti : “ Ndiyenela kukalengeza uthenga wabwino wa ufumu wa Mulungu kumizinda inanso , cifukwa ndi zimene anandituma kudzacita . ” Ndani amacititsa masautso athu ? Cinsinsi Namba 11 Kukhala Wolimbika Sitidziŵa bwinobwino . M’Baibo , liu lakuti “ mtima ” kaŵili - kaŵili limatanthauza munthu wamkati . Motelo ndinalembela kalata a Mboni za Yehova , amene anali kufalitsa mabukuwo , kuti anditumizile mabuku ena . Megan amalalikila uthenga wabwino m’maboti aakulu ndi kwa asodzi ocokela ku Bangladesh , India , Indonesia , Philippines , Thailand , ndi ku Vanuatu . Ndimasangalala kwambili ndikamaceza ndi banja langa Cilengedwe conse , kuphatikizapo anthu , cimagwila nchito motsatila malamulo amenewa . Cimodzi mwa zitsanzo zimenezo ndi ca Loti . ( Mateyu 5 : 1 , 2 ; 7 : 28 ) M’caka ca 33 C.E . , Yesu anakamba ndi ophunzila ake aŵili pamene anali kuyenda pa njila yopita kumudzi wina pafupi ndi Yelusalemu , ndipo ‘ anawafotokozela Malemba momveka bwino . ’ — Luka 24 : 13 - 15 , 27 , 32 . Kusiyana mitundu kwa mahosi kunali kothandiza pofuna kusiyanitsa okwela pa mahosiwo . Ŵelengani Mateyo 13 : 33 . ( Machitidwe 9 : 31 ) Mzimu woyela , umene ni mphamvu ya Mulungu yogwila nchito , ni wamphamvu kwambili . Pamapeto pake mphamvu ya ndalama ya m’dziko lathu inathelatu nchito , ndipo ndinakhala ndilibe akaunti ya ku banki , ndalama za inshuwalansi ndi za penshoni . ” Ndipo ngati sitisamala , tikhoza kucenjenekewa na zinthu monga kufuna kuloŵa nchito yapamwamba yokhala na malipilo ambili , kukhala na umoyo wofewa , kapena kudzionetsela na zimene tili nazo pa umoyo . Imbani mokweza Analimbikitsa Aisiraeli kupilila mavuto amene anali kukumana nawo pamene analoŵa m’dziko Lolonjezedwa . M’nkhani yapita , tinakambilana kuti m’nthawi ya Aisiraeli , anthu amitundu ina analoledwa kulambila Yehova . Koma kuti acite zimenezo , io anafunika kugwilizana ndi anthu a Yehova . ( 1 Maf . Kodi tiphunzilapo ciani pa zocitika zimenezi ? Kumeneko ndi kumvetsa zinthu . Komabe , ambili a ife sindife akulu , conco tingaganize kuti mfundo zimenezi sizingatithandize m’njila iliyonse . Pambuyo pakuti Zekariya waona mpukutu wouluka , mngelo anamuuza kuti ‘ akweze maso ’ m’mwamba . Kodi anthu osamalila okalamba angatsimikize za ciani ? Ngakhale n’telo , ambili a io anapatsidwa cilango cakuti adzakhala m’ndende kwa moyo wao wonse . 3 : 15 ) Koma cokondweletsa n’cakuti Mau a Yehova amatipatsa ciyembekezo cabwino . Cakumbuyo kuli tumapili twa miyala mu mzinda wa makono wa Jaffa , umene unali gombe lakale la ku Yopa Nanga Sara anali na mbali yanji ? Popeza wadzicepetsa cifukwa ca ine , sindidzabweletsa tsokali m’masiku ake . Tsiku lina usiku , atate anabwela kudzanitenga kuti tithaŵe ku Graz cifukwa asilikali a adani anali kuponya mabomba oopsa mu mzindawo . Anthu onse ndikuwagwetsela tsoka ndipo iwe ndidzakupatsa moyo wako monga cofunkha cako kulikonse kumene ungapite . ” ( Yer . Kukhwima kumeneku sikutanthauza kukula kwa kuthupi . M’nkhani yotsatila , tidzaona maumboni ena oonetsa kuti anthu a Mulungu amenewa amalemekeza kwambili Baibo . Nkhani yaciŵili idzafotokoza zifukwa zingapo za m’Malemba zimene zimatilimbikitsa kupitiliza kulalikila mopilila . Tingaonetse khalidweli mwa kukomela mtima munthu aliyense , kulemekeza eninyumba ndi katundu wao , kufikila anthu panthawi imene amapezeka panyumba ndi panthawi imene amakhala omasuka , ndiponso mwa kupeleka uthenga wathu m’njila imene ingacititse eninyumba kukhala ofunitsitsa kumvetsela . Tikamatsatila malangizo amenewa a Yesu , tingacoke pa khomo la mwininyumba tili na mtendele wathu , ndipo timakhala na mwayi wokamulalikilanso m’tsogolo . Kodi mamasulidwe atsopano a Baibo amakuthandizani kuimvetsetsa kapena ayi ? Ndipo tingawathandize motani ? Aja amene akutumikila pa Beteli ndi Nyumba za Misonkhano , amacita nchito yofunika yolalikila uthenga wabwino . Tingaonetse bwanji kuti timayamikila Yehova cifukwa cotipatsa mphatso ya kulankhula ? Ngakhale kuti panali mavuto amenewa , Gayo anapitiliza kutumikila Yehova mokhulupilika . N’zinthu ziti zimene wophunzila Baibo afunika kucita kuti ayenelele ubatizo ? Limodzi mwa mafunso amene ali pamasamba amenewo ndi lakuti : “ Kodi mungapitilize kutumikila Yehova ngakhale makolo anu ndiponso anzanu atasiya kumutumikila ? ” Kodi anaonetsa bwanji kuti atumiki a Mulungu safunika kutengamo mbali m’zandale ? Ngakhale n’conco , ngati makolo ayesetsa kukhomeleza coonadi mu mtima mwa mwana wawo , safunika kudziimba mlandu ngati mwanayo wapanduka . TIYELEKEZELE kuti mufunikila kukakamba ndi wolamulila wamphamvu padziko lonse lapansi , moimilako anthu a Mulungu . Ndimadzifunsa kuti , kodi anthu amaona kuti ndinalephela kuteteza cikwati canga ? ” Motelo , sitiyenela kuona kuti mfundo za m’buku la Yobu zimangogwila nchito kwa odzozedwa amene anapilila panthawi ya Nkhondo Yoyamba ya Padziko Lonse . Cishango ceni - ceni cimene msilikali anganyamule , saizi yake siimasintha , koma cishango cathu cacikhulupililo cingakule kapena kucepa . Zimadalila pa zimene timacita . ‘ Amuna awili opanda pakewo ’ anayamba kupeleka umboni wotsutsana ndi Naboti ndipo iye anaponyedwa miyala mpaka kufa . Mosasamala kanthu za mavutowa , muli na cidalilo camphamvu m’malonjezo a Mulungu ndipo cikhulupililo canu ca tsogolo labwino n’cosagwedezeka . Kodi alipo munthu anaonapo Mulungu , kapena kuonako pamene anali kulenga cinthu ciliconse ? 20 , 21 . ( a ) N’zotulukapo zabwino ziti zimene zimakhalapo ngati tionetsa cikondi cacikhristu kwa anthu othaŵa kwawo ? Nthawi zina mungamve monga mmene wamasalimo anamvela pamene anati : “ Fulumilani , ndiyankheni inu Yehova . Mphamvu zanga zatha . Wophunzila watsopanoyo amayamba kugwilizana nafe m’nchito yokolola ndipo timasangalala kugwilila naye nchito limodzi . — Yoh . 4 : 36 - 38 . MBILI YANGA : NDINALI KUFUNITSITSA KUDZIŴA MAYANKHO A MAFUNSO OFUNIKA KWAMBILI Amai anatumanso foni kwa acibale ao uku akulila , ndipo anali kuwacondelela kuti andithandize kusintha maganizo anga . Koma kodi analapa kucokela pansi pa mtima ? N’ciani cocititsa cidwi ndi mmene Mulungu anayanjila mafumu anayi aciyuda ? Cotelo anapanga shopu yogulitsa aisi kilimu , koma ndalama zitamuthela anangotseka shopuyo . Amazipatsa Yehova zilizonse zimene zifunikila . 7 : 39 ) Akristu amene amakwatila kapena kukwatiwa kwa Mkristu mnzake , amapeza bwenzi lodzipeleka kwa Yehova ndipo limawathandiza kukhalabe okhulupilika kwa Mulungu . Kodi mumayamikila zimene Yehova anakucitilani ? Ifenso Akhristu masiku ano , tili monga alendo m’dzikoli , limene n’lodzala na makhalidwe oipa ndiponso kulambila konama . Anthu asoceletsedwa na Babulo Wamkulu , ufumu wa cipembedzo conama , komanso “ malo okhala ziwanda . ” ( Chiv . M’caka ca 2000 , n’nakwatila Karolin , mlongo wokongola amene amakonda Yehova mmene ine nimam’kondela . Mzimayiyu anasankha kungouzidwa zocita , m’malo moseŵenzetsa mphatso yabwino kwambili imene Mlengi wake anam’patsa . Inde , mphatso ya ufulu wosankha wekha zocita . N’cifukwa ciani Yesu anafotokoza fanizo la matalente ? Zinthu zonse zimene ndikupanga n’zatsopano . ’ ” Monga mmene ulosiwu unanenela , Aisiraeli anakhala akapolo kwa nthawi yaitali . Kwangotsala pang’ono kuti tiloŵe m’dziko latsopano lolungama . Ife atumiki a Yehova sitipusitsidwa mwa njila imeneyi . N’cifukwa ciani timadana ndi imfa ? ( Ŵelengani Chivumbulutso 12 : 9 , 12 . ) Iye anali ndi mphamvu zocilitsa ndi zoukitsa anthu , koma anali kuvutikabe ndi matenda . Tinaphunzila kuti Yehova ndiye Mlengi wathu ndi Wotipatsa Moyo , ndipo ali nafe na colinga . Conco , tikamakonda kwambili Yehova , Mwana wake , Akhristu anzathu , ndi anthu ena , timaonetsa kuti ndise okhwima mwauzimu . — Mat . Abulahamu anaonetsetsa kuti mwana wake Isake akwatile mkazi wolambila Yehova . Koma kwenikweni ana samaonetsa cidwi kaamba kakuti kholo lao linali kwina nthawi yaitali . N’nakaikila zimene anakamba , koma n’naganiza zoŵelenga Baibo kuti nipeze mayankho . Basi iye n’kupeleka nsembe kwa Mulungu , cinthu cimene sanali kuloledwa kucita . Kodi kuganiza bwino kugatithandize bwanji kusankha mwanzelu pankhani ya cithandizo ca mankhwala ? Coyamba , timadziŵa kuti zimene timaphunzitsa ndi coonadi cifukwa zimacokela m’Baibulo . ( Aroma 7 : 24 , 25 ; 1 Yohane 2 : 1 , 2 ) Kumbukilani kuti Yesu anafela anthu olapa . Kodi tiyenela kuwaona bwanji abale ndi alongo athu ? Koma popeza n’nali mwana , sin’nali kudziŵa kuti kukhala nilibe manja kudzakhudza bwanji umoyo wanga . 16 : 12 ) Koma izi sizitanthauza kuti palibe ciliconse cimene tidziŵa ponena za nthawi imene akufa adzauka . 30 : 20 , 21 ) Masiku ano , okwatilana ‘ angamvele ’ mau a Yehova mwa kuŵelengela pamodzi Mau ake . CIZINDIKILO CA MASIKU OTSILIZA Ulosi wa m’Baibulo umatithandiza kudziŵa cimene cimacititsa mavuto ena amene akhala akucitika m’dziko monga Nkhondo Yoyamba ya Padziko lonse . Izi zinali kumupweteka kwambili mumtima . ( Ŵelengani 1 Petulo 1 : 22 ; Luka 22 : 24 - 27 . ) Ndinabadwila m’dziko la France , kum’maŵa koma cakumpoto kwa dzikoli mum’zinda wa Mulhouse , umene unali kudziŵika cifukwa ca ciwawa . Yehova angakuthandizeni kupanga zosankha mwanzelu mukali acinyamata . N’tafika zaka 20 , n’nakwatila . Koma patapita nthawi yocepa amai ake anamwalila . Wosimba ni Erika Nöhrer Bright 32 : 4 ) Tikamudziŵa kwambili Yehova , timayamba kumukonda kwambili ndi kukondanso njila zake , cakuti sitingafune kuti nthawi zonse tizidziŵa cifukwa cake amacita zinthu mwa njila inayake . Baibulo limati : ‘ Yesu . . anazunzika mpaka imfa kuti mwa kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu , alaŵe imfa m’malo mwa munthu aliyense . ’ — Aheberi 2 : 9 . Koma ndiye mmene tifunika kucitila ngati tifuna kucilikiza ulamulilo wa Yehova . ( Aef . 5 : 22 , 23 ; 6 : 1 - 3 ; Aheb . Cisoti cimene msilikali waciroma anali kuvala cinali kuteteza mutu wake , khosi , na nkhope yake ku zida za adani . Pa ubatizo wake , Yesu anamvela mau ocokela kumwamba akuti : “ Uyu ndiye Mwana wanga wokondedwa , amene ndimakondwela naye . ” ( Mat . Conco , sitingayembekezele kuti abale athu azikamba kapena kucita zinthu zabwino zokhazokha . Zosankha zathu zimakhudza umoyo wathu . Mulungu sadzalekelela anthu amene amaphwanya lamulo lake limeneli mwadala . — Aheb . Anakambanso kuti : “ Umoyo wosafuna zambili umandikondweletsa cifukwa wandithandiza kuika maganizo anga pa zinthu za kuuzimu . ” Iye ndi “ Wakumva pemphelo . ” ( Sal . Anamasulidwa m’ndende ndi kuikidwa pa udindo pambuyo wapamwamba kwambili wokhala waciŵili kwa mfumu ya Iguputo . — Gen . Mwacitsanzo , mu 73 B.C.E . , Spartacus , wocita maseŵela omenyana ndi anthu kapena nyama , pamodzi ndi akapolo 100,000 anaukila boma la Aroma koma sanapambane . Padziko lonse , ciŵelengelo ca anthu othaŵa kwawo cifukwa ca nkhondo kapena cizunzo , tsopano cipitilila 65,000,000 . Mulungu analenga anthu ndi ufulu wosankha . Mwina tingaganizile munthu amene akuyesetsa kuti athyole cipatso cokongola colendewela mu mtengo . Laura anati : “ Imeneyo inali nthawi yanga yoyamba kuthela nthawi yambili mu ulaliki , ndipo ndinakondwela kwambili . ” Acibale anga okwana 13 anali kugwila nchito pa chalichi ndipo ena pakati pao anali ansembe . Ricky ndi mkazi wake Kendra , ndi okondwela kwambili , osati cabe cifukwa cakuti akutengako mbali pa nchito yomanga ku Warwick , koma cifukwa cakuti kusamuka kwao kwathandiza kuti mwana wao akule mwa kuuzimu . — Miy . Baibulo limati : “ Yehova anapitilizabe kukhala ndi Yosefe ndi kumusonyeza kukoma mtima kosatha . Ndipo anacititsa mkulu wa ndende kum’konda Yosefe . ” ( Aroma 12 : 4 - 8 ) Yehova watipatsa udindo , umenenso ni umboni wakuti amatidalila na kutilemekeza . — Ŵelengani 1 Petulo 4 : 10 . Mau a Mulungu amati : “ Mtima umadziŵa kuŵaŵa kwa moyo wa munthu , ndipo mlendo sangaloŵelele pamene mtimawo ukusangalala . ” ( 2 Tim . Yehova anam’gwilitsila nchito Amosi ngakhale kuti poyamba anaoneka kuti analibe luso locita zinthu zina . — Amosi 7 : 12 , 13 , 16 , 17 . Koma mwatsoka lanji , atate anamwalila . ( Mat . 10 : 11 - 13 ) Timayamikila ngati ena alemekeza nyumba ndi katundu wathu . Iye ananena kuti nthawi zina anali kukopeka ndi akazi amene sanali a Mboni . Mumamva bwanji kuti Yesu anapeleka mtengo wa magazi ake kwa Yehova ? Kupyolela mu pangano limenelo , mtundu wakale wa Isiraeli unakhala mtundu wa Mulungu wosankhidwa . [ Mau apansi ] Kuti mudziŵe zambili ponena za maulosi amenewa , onani nkhani 3 m’buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa yofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . [ Cithunzi papeji 4 ] N’natsitsimukila m’selo yozizila kwambili imene munalibe cakudya , madzi , kapena bulangete . Pitilizani kutumikila Yehova . Tikayang’ana cilengedwe ca Yehova , timaona umboni wakuti iye amatikonda kwambili . Kodi Paulo anawathandiza bwanji Akhiristu a ku Korinto kukhala ndi kapenyedwe ka Mulungu pa nkhaniyo ? Nanga kudziŵa zimenezi kuyenela kukhudza bwanji zinthu zimene timaika patsogolo , mmene timaseŵenzetsela Intaneti , ndi mmene timasankhila anzathu na zosangalatsa ? 136 : 1 ) Mu Salimo 136 , mau akuti “ kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale ” amachulidwa nthawi 26 . Pamene mapeto a dziko la Satana akuyandikila , gulu la Yehova padziko lapansi likupita patsogolo kwambili . ( Aroma 3 : 23 ) Conco , sitiyenela kupatsa munthu wina aliyense ulemu wopambanitsa ngati kuti tikumulambila . 56 : 8 . 15 : 14 . Iye atazindikila kuti mwamuna wake sanali kudziŵa zenizeni zokhudza ciphunzitso ca Utatu , mwaluso anamufunsa kuti : “ Kodi mumakhulupilila kuti Mulungu ndi Mulungu , Yesu naye ndi Mulungu ndi kuti mzimu woyela naonso ndi Mulungu ; ndiponso kuti io si Milungu itatu koma ndi Mulungu mmodzi ? ” Pamene ticita izi , tiyenela kukumbukila kuti colinga cimene timaŵelengela Baibo si kungofuna kukhala na cidziŵitso . Koma pa cocitikaci , n’nadzionela nekha za ubalewu . Tinaganiza zogwilitsila nchito luso lathu mwa kutsegula sukulu yophunzitsa kuvina kuti tizisamalila banja lathu . Ndiye cifukwa cake , nthawi zonse tiyenela kugwilitsila nchito Mau a Mulungu cifukwa ndi amoyo . N’ciani cinacititsa kuti akhale na colinga cimeneci ? Ndi kusintha kotani kokhudza gulu lathu kumene kunapangidwa ca m’ma 1970 ? “ Ananu , . . . mvelani malangizo kuti mukhale anzelu . ” — MIY . ( Yak . 4 : 8 ) ‘ Kapena nifuna kusamuka n’colinga cakuti makolo anga asamaone zimene nimacita kapenanso kuti nisamakhale na zocita zambili ? ’ Mneneli Yesaya anakamba kuti “ m’masiku otsiliza , ” anthu ocokela ku mitundu yosiyanasiyana adzabwela pamodzi kuti alambile Yehova . Komabe , Baibulo landithandiza kudziŵa kuti ngozi imeneyo siinali cilango cocokela kwa Mulungu . Yehova amacita zinthu modziletsa nthawi zonse cifukwa nchito zake zonse n’zangwilo . ( Deut . Komabe , iye anapitilizabe kulemekeza Davide . Kuonjezela pamenepo , Abisai anali mkulu wa asilikali ndipo akanafuna akanadziika kukhala mfumu , koma sanacite zimenezo . Sachio na Mizuho M’malo mwake , ‘ mdulidwe wao ndi wa mumtima wocitidwa ndi mzimu . ’ — Aroma 2 : 29 . “ Tipita Nanu Limodzi , ” Jan . UBONGO wa munthu ndi wapadela kwambili . Mbonizo zitacoka , ndinayendetsa galimoto pa mtunda wa makilomita 56 kupita ku sitolo kogulitsa mabuku acikristu . Tizikumbukilanso kuti m’maiko ambili anthu oculukilaculukila akulandila coonadi . Anthu oyamba kupanga mtundu watsopano wa Mulungu anali atumwi ndi ophunzila ena a Kristu oposa mahandiledi . Masiku ano , Akristu ambili a zaka za m’ma 50 kapena kuposelapo amaona kuti umoyo wao wasintha ndi kuti angatumikile Yehova m’njila zina . ( Aroma 10 : 12 ) Yehova watiphunzitsa kuti tizikondana monga abale . Ca m’ma 167 B.C.E . : Mfumu yaciselukasi dzina lake Antiyokasi Epifanasi , amene anali kukakamiza Ayuda kuyamba cipembedzo ca Cigiriki , analamula kuti mipukutu yonse ya Malemba a Ciheberi iwonongedwe . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Iwe amene umalalikila kuti ‘ Usabe , ’ umabanso kodi ? ” — Aroma 2 : 21 . Kusonkhanitsa kumeneku kudzacitika panthawi imene otsalila a 144,000 adzalandila mphoto yao yakumwamba . ( 1 Ates . 4 : 15 - 17 ; Chiv . Kodi kucita zimenezi n’kopepuka ? Popeza kuti anali atafa kale , zinali zosatheka kumulanga . Mwacitsanzo , pamene ciwawa cinafala mu Isiraeli , Mulungu anauza mneneli wake Yesaya kuti auze anthu kuti : “ Ngakhale mupeleke mapemphelo ambili , ine sindimvetsela . Manja anu adzaza magazi amene mwakhetsa . ” 6 : 19 , 20 , 24 . Coyamba , cifukwa munaŵelenga Baibulo lonse . Tikangodziŵa zilakolako zimenezo , ndi bwino kucitapo kanthu kuti ‘ tisagwidwe amoyo ndi [ Satana ] pofuna kukwanilitsa colinga cake . ’ ( 2 Tim . Ndi zitsanzo ziti za m’Baibo za anthu amene anatumikila kumalo osoŵa zimene zingalimbikitse Akristu acikulile masiku ano ? Komabe , zinthu zabwino - bwino zimenezi si zimene atumiki a Mulungu anaziika patsogolo kwambili mu umoyo wawo . Timoteyo akumwetulila pamene akuganizila amai ake ndi agogo ake , amene akumunyadila uku akupukuta misozi pamene iye akucoka . Kodi Yesu analimbikitsa bwanji ophunzila ake tsiku limene anaukitsidwa ? ( Yobu 31 : 1 ) Koma kumbukilani kuti pa nthawiyo , Mulungu anali kulolela anthu kukwatila cipali . Akalonga a Farao anaona kuti Sara anali wokongola kwambili , ngakhale kuti panthawiyo anali wacikulile . Aliyense wa ise anaitaniwa kuti akhale bwenzi la Mulungu na Mwana wake . Zimenezi zikusonyeza kuti wodzozedwa aliyense ali ndi ufulu wosankha kukhala wokonzeka ndi kukhala maso , kapena kukhala wopusa ndi wosakhulupilika . ( Miy . 27 : 11 ) Conco , ngati timvela Yehova mokhulupilika , ndiye kuti tikum’patsa cinthu camtengo wapatali cimene amakondwela naco . Koma kodi pali cifukwa comveka comangoganizila zimenezi ? Suntuke sanaitanidwe , koma anamvela kuti kumeneko kunali maceza acisangalalo . Paulo anadziŵa kuti panali zambili zimene sakanakwanitsa kucita popanda thandizo locokela kwa Mulungu . ( 1 Akorinto 14 : 25 ) Pali maumboni ambili oonetsa kuti Mulungu ali ndi anthu ake . Kudziŵa malemba oyela n’kofunika . Ngakhale kuti sitidziŵa zonse zimene zidzacitika pa nthawi yaciyeso imeneyo , n’zoonekelatu kuti tidzafunika kukhala ndi mtima wodzimana kwambili . Pa cifukwa cimeneci , Mkhristu akayamba kukhwima mwauzimu , amayambanso kuona kuti kukonkha mfundo za m’Baibo n’kofunika kwambili . Monga mmene Iye wathandizila anthu amenewa , “ Mulungu amene amapeleka ciyembekezo akudzazeni ndi cimwemwe conse ndi mtendele wonse cifukwa ca kukhulupilila kwanu . ” — Aroma 15 : 13 . Ndipo n’zacisoni kuti okalamba ambili amanyalanyazidwa panthawi imene afunikila cisamalilo cacikulu . — Sal . ( Aroma 6 : 23 ) Kodi pali cimene tinacita kuti tilandile dalitso limenelo ? 12 : 7 - 12 . Rute anapita nawo limodzi ku Isiraeli . Cidalilo cathu mwa Yehova cidzakula ngati tikumbukila mfundo yakuti iye angathe “ kucita zazikulu kwambili kuposa zonse zimene timapempha kapena kuganiza . ” — Aef . Baibulo limakamba kuti “ amuna 10 ” “ adzagwila covala ca munthu amene ndi Myuda ndi kunena kuti : ‘ Anthu inu tipita nanu limodzi , cifukwa tamva kuti Mulungu ali ndi inu . ’ ” Tisamakhwethemuke tikakumana ndi zovuta pali pano . ( Salimo 33 : 11 ) Kukamba zoona , ngati tiphunzila kuona zinthu mmene Yehova amazionela , tidzasankha zinthu mwanzelu ndipo tidzacita zinthu zom’kondweletsa . Kwa io moyo ungakhale masiku a mdima okha - okha . — Mlal . Mtumwi Paulo anaticenjezelatu kuti ‘ m’masiku otsiliza ’ zinthu zidzakhala ‘ zovuta . ’ ( a ) Kodi kukhala na zolinga zauzimu kumakhudza bwanji ubwenzi wathu na Yehova ? Anakhalabe wokhulupilika ndi womvela mpaka imfa yake . Akanacititsanso kuti tileke kukhala ndi zilakolako zoipa . Rabeka anali wodzicepetsa , khalidwe lofunika kwambili 10 : 13 ) Ndi masautso otani amenewo ? Koposa zonse , mudzakhala wokondwela podziŵa kuti mwapeza cinthu camtengo wapatali kuposa golide . — Miy . N’cifukwa ciani tatsindika conco ? Yesu anakamba kuti , mumtima mumacokela “ maganizo oipa , za kupha anthu , za cigololo , za dama . ” — Mat . Mmalomwake , anayelekezela Goliyati ndi Yehova . Tiyeni tikhalebe okhulupilika kwa Yehova mofanana ndi Davide , Yonatani , Natani , ndi Husai . Tikatelo tidzakhala ndi umoyo wosangalala . “ Mtima wa munthu wolungama umayamba waganiza usanayankhe , koma pakamwa pa anthu oipa pamasefukila zoipa . ” ( Miy . Maka - maka Akhristu acicepele ndiwo amaoneka kukhala osatetezeka . Ni mwayi waukulu kwambili ‘ kudziŵidwa ndi Mulungu , ’ Wolamulila Wamkulu wa cilengedwe conse . Njila imodzi yaikulu imene tingacitile zimenezo ndiyo kuganizila mozama za dipo . Mng’ono wanga anali ndi ufulu wolankhula nao , kuwakumbatila ndipo anali kuwakonda kwambili , koma ine ndinali wotalikilana nao . Cozizwitsaci cikuonetsanso kuti Yesu ndi wacifundo . Kodi tingaonetse bwanji Khalidwe Lopambana polalikila ? Koma osati cifukwa cakuti anali wokalamba . Koma sikuti tidzapulumuka cabe cifukwa cakuti tili m’gulu la Mulungu . Komanso , makampani ambili amafuna kupanga zinthu zambili olo kuti ali na anchito ocepa . Kucita zimenezo kudzakuthandizani kudziŵa mmene mungafotokozele ena zimene mumakhulupilila . Ni ngozi yanji imene otsatila a Khristu angakumane nayo masiku ano ? N’COFUNIKA KWAMBILI KUTI MUNTHU AKHALE PA UBWENZI WABWINO NA MULUNGU . MAKOLO acikhristu akuyang’ana mwana wawo wamkazi wacicepele , amene tam’patsa dzina lakuti Maria . Komabe , iye anakamba kuti : “ Mulungu [ adzanipulumutsa ] kudzela mwa Yesu Khristu Ambuye wathu . ” ( 2 Akorinto 8 : 4 ; 9 : 7 ) Paulo sanali kutanthauza kuti iwo anacita zopeleka cifukwa cakuti anali ndi cimwemwe , koma kuti anali na cimwemwe cifukwa copatsa . Yehova amalamula atumiki ake kukwatiwa “ mwa Ambuye . ” ( 1 Akor . Ganizilani zimene Yehova anauza Aisiraeli ponena za anthu amene sanali kum’tumikila . Koma comwe unali kufuna cikacitika cimakhala ngati mtengo wa moyo . ” — Miy . Kwa zaka 6 , Elisa anali kuyenda ndi mneneli wacikulileyo ndi kumuthandiza pa nchito yake . Ifotokozanso mmene Mulungu waonetsela cikondi ku mtundu wa anthu . Mwacitsanzo , Yunike mkazi waciyuda amene anakwatiwa ndi mwamuna wacigiriki wosakhulupilila , pamodzi ndi amai ake a Loisi , anamvetsela mosamalitsa kwa Paulo ndi Baranaba . Koma ngati timaona kuti kucilikiza ucifumu wa Yehova n’kofunika , cidzakhala cosavuta kupilila mavuto amene timakumana nawo tsiku na tsiku . ( a ) Kodi Samueli anamva bwanji pamene Aisiraeli anamuuza kuti afuna mfumu ? Odala ndi anthu onse amene amamuyembekezela . ” Fumiko , amene anapulumuka mphepo yamkuntho ku Japan , anati : “ Mapeto ali pafupi kwambili . Koma iye anasungabe lumbilo lake . Pangano la mu Edeni litsimikizila kuti Yehova kupyolela mwa mbeu ya mkazi , adzakwanilitsa cifunilo cake ponena za dziko lapansi ndi anthu . Cina cimene cingatithandize kudziŵa mmene Yehova amaonela zinthu , ndi kumvetsela mwachelu zimene gulu lake limaphunzitsa kucokela m’Baibulo . M’zaka 100 zapitazi , anthu odzicha Akristu ndi amene akhala akucita zimenezi . A Mboni za Yehova ambili anakwanitsa kuthetsa maganizo olakwika amene anali nawo pa zandale . 2 : 9 ) Ndithudi , pangano latsopano n’lofunikadi ! Nthawi zina , sitingamvetse cifukwa cake munthu wina mumpingo angasankhe mosiyanako pankhani inayake yaumwini . Tiyeni tione zitsanzo ziŵili izi : Tsiku lina pamene ophunzila anali kuyenda na Yesu m’dela la Asamariya , anapempha malo ogona m’mudzi wina kumeneko . Daniel anatsala pan’gono kukomoka cifukwa colema . Maureen Kumapeto kwa zaka za m’ma 1300 C.E . , John Wycliffe wa ku England anayamba kumasulila na kutulutsa Baibo m’Cizungu cimene ngakhale anthu wamba anali kumvela . Ndipo kuŵelenga malemba ambili - mbili kungacititse kuti omvela asagwilepo mfundo iliyonse pa malembawo . ( Eks . 3 : 12 ) Caciŵili , Yehova anam’patsa cidalilo mwa kumuuza tanthauzo la dzina lake kuti : “ Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala . ” * ( Eks . N’cifukwa ciani sitifunika kutenga mbali m’ndale ? Iye anati : “ Pamene maganizo akhala pansi , nkhawa zonse zimaloŵedwa m’malo ndi mphamvu ndiponso cikondi ca Yehova . Kenako , tidzakambilana zimene tingaphunzilepo pa zitsanzo za anthu ochulidwa m’Baibo amene anali odziletsa ndi amene anali osadziletsa . Ndi vuto liti limene silidzatha m’dziko loipali ? 22 : 32 ) Ngakhale lomba , tikulandila madalitso ambili . Hutter anamasulila bwino kwambili Malemba Acigiriki Acikhristu m’Ciheberi . KWA zaka zambili , Kevin anali kuchova njuga , kukoka fodya , kuledzela , ndi kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza ubongo . N’zoona kuti kugwila nchito yolemetsa si kopepuka . Paulo anagwilitsila nchito citsanzo ca thupi pofotokoza kuti Mkristu aliyense angathandize kuti mpingo ukhale wogwilizana ndi kutsatila Yesu amene ndi Mtsogoleli wa mpingo . Onaninso zimene Salimo 106 : 32 , 33 imakamba . Imati : “ Iwo anaputa mkwiyo [ wa Mulungu ] pa madzi a ku Meriba , moti Mose sizinamuyendele bwino cifukwa ca anthu amenewa . ( 2 Timoteyo 3 : 1 - 4 ) N’zoona kuti kusalemekeza anthu sikwacilendo , koma zimenezi zacita kunyanya “ masiku otsiliza ” ano amene akuchulidwa kuti “ nthawi yapadela komanso yovuta . ” Komabe , mwina tingadzifunse kuti : ‘ Kodi izi zitanthauza kuti nifunika kuyembekezela kwa nthawi itali kuti nikaonane na okondedwa anga amene anamwalila ? Doreen anati “ N’naphunzila kuti siniyenela kukana thandizo iliyonse . ( Mat . 23 : 23 , 24 ) Koma ngati tipeleka ulemu woyenelela kwa olamulila a boma , pangakhale zotulukapo zabwino , mwinanso zimene sitinali kuyembekezela . ( Mateyu 5 : 37 ) Samalani kuti musamange mfundo zimene mudzalephela kutsatila . Sanakaikile ngakhale pang’ono malonjezo a Mulungu . Anthu masiku ano ndi “ osafuna kugwilizana ndi anzawo , ” ndiponso “ osamva za ena , ” ndipo mtsogolomu adzakhala ogaŵikana kwambili . Penti wofiilila wokwela mtengo anali kuutenga ku nkhono zina . Zinthu monga zomela zosiyanasiyana , mizu , masamba , ndiponso tudoyo , zinali kugwilitsidwa nchito kupangila penti wofiila , wacikasu , wabulu , ndiponso wakuda . ( Yer . Ena angaganize kuti kumeneku n’kusiyana pakati pa anthu ali m’coonadi ndi amene salimo , komanso pakati pa Akhiristu ndi anthu akunja . Iye analimbikitsa mtendele , anadyetsa anthu ambili mozizwitsa , anacilitsa odwala , na kuukitsa akufa . — Mateyu 12 : 15 ; 14 : 19 - 21 ; 26 : 52 ; Yohane 11 : 43 , 44 . Atate anga anali membala wacangu wa cipani ca Nazi , ndipo anali dilaiva wa mtsogoleli wa cipani ca Nazi m’dela lathu . Acinyamata ndi acikulile , onse amalakwitsa nthawi zina . ( 1 Pet . Pa cifukwa cimeneci , anthu ambili sakhutila ndi zimene ali nazo . Pamene fanizo la Yesu la matalente likukwanilitsidwa nthawi ino ya mapeto , kodi otsatila ake akuigwiladi nchito imeneyi ? Izi zinan’thandiza kuzindikila kuti ni khalidwe loipa . Pa mwalawu panali dzina la Pilato m’Cilatini “ Anapitiliza kupilila moleza mtima ngati kuti akuona Wosaonekayo . ” — AHEB . Ngakhale kuti Solomo anali Mfumu yanzelu , “ anali kusinkhasinkha ndi kufufuza zinthu mosamala ” n’colinga cakuti zolemba zake zikhale zolondola ndi zosangalatsa . Kucita zimenezi kungatenge nthawi yaitali . ( Luka 10 : 25 - 37 ) Pamenepa , Yesu anaonetsa kuti Msamariya akanatha kuphunzitsa Ayuda mmene akanaonetsela cikondi ceni - ceni kwa anzawo . Iye sanataye mtima . Kukamba zoona , nthawi zina cimavuta kusankha zovala mogwilizana ndi mfundo za Mulungu . M’mashopu ambili amagulitsa zovala zamasitayelo amene afala . M’nkhani yotsatila tidzakambilana mfundo za m’Malemba zothandiza Akhiristu ali pabanja mmene angacitile ndi mavuto a “ masiku ano otsiliza . ” Maka - maka pamene amuna ndi akazi ambili ali na makhalidwe osoŵetsa cimwemwe m’mabanja awo . ( 2 Tim . 17 , 18 . ( a ) N’ciani cimene Akristu amasankha kucita nthawi zonse ? ( b ) Nanga mungawathandize bwanji kuyamba kukonda utumiki ? Musakayikile kuti panthawi ina yoyenelela , iye adzakuthandizani . Nditaona zikhalidwe zosiyanasiyana ndi mabungwe osiyanasiyana , ndinakhala wotsimikiza mtima kuti cinthu cabwino kwambili cimene ndingacite paumoyo wanga ndi kuzungulila dziko lapansili lokongola , anthu asanaliononge . 17 : 17 ; Yoh . 15 : 15 . Chris anauza Gavin kuti m’Baibulo muli uthenga wofunika kwambili , ndipo kuphunzila uthengawo kungamuthandize kupindula ndi misonkhano . 17 , 18 . ( a ) Kodi anthu a Yehova adzalandila malangizo otani Gogi akadzawaukila ? Masiku otsiliza adzatha pamene zoipa zonse zidzacotsewapo . — 1 Yohane 2 : 17 . 1 Samueli caputa 1 - 2 Zinali zokondweletsa kum’thandiza mwanjila imeneyo kufikila pamene anatsiliza moyo wake wa padziko mu December 1992 . Kodi anthu amene afedwa tingawatonthoze bwanji ? 6 : 13 - 18 ) Kwa Nowa , Yehova anaonetsadi kuti ni Mulungu wa cilimbikitso . Ambili a ife tingavomeleze kuti kucita zimenezi n’kosavuta , ndipo kumangofuna kupatula nthawi . N’NABATIZIKA nili na zaka 15 . Maboma ena ndi ankhanza . ( b ) Tingapewe bwanji kucimwila Yehova ? Kodi nimam’pempha mzimu woyela na nzelu kuti zinithandize kucita zinthu zom’kondweletsa ? — Sal . Ndipo ndife otsimikiza mtima kuti iye adzapitilizabe kutelo , ngakhale kuti sitidziŵa mmene adzacitila zimenezi . ” — Sal . Anthu okoka fodya komanso amene sakoka , amaononga ndalama zambili pofuna thandizo ku cipatala . Kodi Khalidwe Lopambana n’ciani ? Umu ndi mmene Yehova amawaonela . Mwacitsanzo , khalidwe limeneli limayendela pamodzi ndi kupilila , kumene kumatithandiza kuona zinthu moyenela ndi kukhala wolimba pamene tikumana ndi mavuto . ( Akol . Iye anati : ‘ Iwo sanafune kumudziŵa Mulungu molondola . ’ Iye anati : “ Palibe cimene cimandisangalatsa kwambili kuposa kumva kuti ana anga akuyendabe m’coonadi . ” — 3 Yoh . 4 . Mwacitsanzo , Yehova anam’khululukila Aroni pa zimene anacita . Koma kumene mwapita mwapeza mzela wautali kuposa umene mwasiya . ( a ) Kodi Yesu anaphunzitsa bwanji ophunzila ake kukhala odzicepetsa ndi kupewa kudzikonda ? Ofalitsa 215 ndi apainiya 28 a m’mipingo itatu ya m’mudziwo , anasangalala kwambili pamene anthu 1,600 anapezeka pa Cikumbutso mu 2014 5 : 6 - 9 ) Tiyeni tikambilane njila zitatu za mmene tingacitile zimenezi . Kucokela apo , Aaron anali kucita upainiya mokondwela ndi kugwila nchito pamodzi ndi ena amene amathandiza pakacitika ngozi . ( 1 Tim . 2 : 9 , 10 ) Conco akakhala pa gulu , cimakhala covuta kusiyanitsa pakati pa munthu amene ali ku mbali ya Yehova ndi amene ni ‘ bwenzi la dziko . ’ — Yak . Ngakhale kuti Mulungu amaona kuti mwamuna ndi mkazi ndi ofanana , Baibulo limakamba kuti aliyense wa io ali ndi udindo wake m’banja . ( Chivumbulutso 16 : 14 - 16 ; 19 : 14 - 16 ) Angelo amphamvu adzatumikila monga akupha pa ciweluzo ca Mulungu , pamene Ambuye Yesu “ adzabwezela cilango kwa anthu . . . osamvela uthenga wabwino wonena za Ambuye wathu Yesu . ” — 2 Atesalonika 1 : 7 , 8 . Eliya anapindula ndi thandizo la Yehova , ndipo anayambanso kugwila nchito ndi mphamvu . — 1 Maf . Conco , tiyeni tione zimene tingaphunzile pa zitsanzo za Nowa , Davide , ndi atumiki ena okhulupilika a Yehova amene anam’dalila na kucitapo kanthu . Itionetsanso mmene tingaonetsele ndi kulimbitsa cikhulupililo cathu . — Aheberi 11 : 6 . 4 : 30 ) Iwo ayenela ‘ kuongola njila zimene mapazi ao akuyendamo . ’ — Aheb . 10 : 23 ) Koma ngati tidalila citsogozo ca Mulungu tidzapambana . Kodi m’bale wina wacicepele analimbikitsiwa bwanji pa nthawi yovuta ? Mukacita zimenezo , mudzakhala woyenela kubatizidwa . Coyamba , kugwila nchito mwakhama kumatithandiza kupeza zofunikila pa umoyo . Kutumikila Yehova ndiye njila yabwino imene tingapezelemo cimwemwe . Mtumwi Paulo anaonetsa kuti anali kulemekeza moyo mwa kucitila umboni mokwanila . Kuwonjezela apo , Nowa anaonetsanso cikhulupililo cake mwa kukhala “ mlaliki wa cilungamo . ” — Gen . Ataona kuti wakana kusintha maganizo ake , anayelekeza monga afuna kumupha . 14 , 15 . ( a ) Kodi Yehova anamva bwanji pamene Eliya anacita mantha ? NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO Mphamvu ya Imfa 3 Ayi . Coyamba dzifunseni kuti , ‘ Kodi kugwilizana nawo kudzakhudza bwanji ubwenzi wanga na Yehova ? Iye anapepesa kwa mlongo wake ndi kum’kumbatila . ” Anthu akandiona ndikubwela , anali kuthaŵa . Koma n’nali na vuto linalake . ” Ndiyeno , amafufuza m’Baibulo ndi m’zofalitsa zathu kuti apeze mfundo zimene zingatithandize . CINANSO CIMENE MUNGACITE : Kodi zikukuvutani kudziŵa zimene mumacita bwino ? Ena amalalikila , koma amacita zimenezi kwa nthawi yocepa . 3 : 6 , 17 ) Mdyelekezi anakamba bodza . amathamangila pa mbali ‘ yofunsa munthu mafunso . ’ ” Mwacitsanzo , pomanga likulu lathu latsopano ku Warwick , mu mzinda wa New York , abale na alongo 27,000 anadzipeleka kuti athandize pa nchitoyo , ena kwa mawiki aŵili , caka kapena kuposelapo . Mpake kuti McClintock na Strong anati : “ Kukondwelela Khrisimasi sikunacokele kwa Mulungu , ndipo sikucokela m’Malemba a Cipangano Catsopano . ” Pangano latsopano limayala maziko a anthu amene adzakhala “ olandila coloŵa anzake a Kristu . ” Ndikaŵeluka kusukulu , ndinali kukonda kudyesela nkhuku ndi kutola mazila ake , komanso kusamalila ng’ombe ndi nkhosa . Ngati Yesu sanaukitsidwe , ndiye kuti Uthenga wabwino wonena za munthu wabwino ndi wanzelu , amene anaphedwa ndi adani ake ndi wopanda phindu . Ndipo anthu onse ayenela kudziwa mfundo ya coonadi yofunika kwambili imeneyi . Pofotokoza zocitika za m’buku la Ezekieli caputala 1 , iye anakamba zimene anaphunzilapo mwa kunena kuti : “ Yehova amatsogolela galeta lake , gulu lake pa liŵilo limene iye afuna . Paulo ndi Baranaba anayenda okha kudutsa malo oopsa . ( Mac . Kucita izi n’kofunika kwambili kuti tikhale pa ubwenzi wolimba ndi Yehova . ( Luka 8 : 18 ) Mwacitsanzo , ndi kupanda nzelu kupempha Yehova kuti atithandize kukaniza cilakolako ca ciwelewele , koma kwinaku tikupenyelela zamalisece kapena mafilimu a ciwelewele . Tiphunzilapo ciani pa fanizo la matalente ? ( a ) Kodi Satana angagwilitsile nchito bwanji mtima wathu kuti atisoceletse ? Malembawa amanena kuti nkhondo , njala , matenda ndi imfa zidzatha . Cikumbutso citatsala pang’ono kucitika , komanso maka - maka pa nthawi ya cikumbutso yeni - yeniyo , yesetsani kuganizila mozama za tanthauzo la mkate wopanda cofufumitsa ndi vinyo wofiila . ( 1 Akor . Pakacitika Zinthu Zimene Zingasokoneze Ubwenzi , Mar . Conco , Yehova anauza Mose kuti : “ Ndodo iyi izikakhala m’dzanja lako kuti ukaigwilitse nchito pocita zizindikilo . ” Paulendo wa Aisiraeli wa m’cipululu , Kora , Datani , ndi Abiramu , anapandukila ulamulilo wa Mose ndi Aroni . ( Onani cithunzi cili kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) N’ciani cinacitikila anthu onse opanda cikhulupililo m’nthawi ya Nowa ? Akulu anzake amaona kuti Dannykarl ndi mkazi wake Jennifer , ni dalitso mumpingo wawo . ( Mlal . 5 : 10 ) Koma pali njila imene tingapewele vuto la kukonda cuma . Tifunika kumaphunzila Mau a Mulungu , Baibo , tsiku lililonse . Panali kudzakhala nkhondo , njala , ndi milili . ( 2 Ates . 3 : 2 ) Komabe , Yehova wapatsa mlambili wake aliyense “ cikhulupililo . ” ( Aroma 12 : 3 ; Agal . Pocita zimenezo anapatsa anawo shuga , mkaka , na masamba a khofi . Mwacitsanzo , anthu ambili amaona kuti si kulakwa kugonana ndi mwamuna kapena mkazi mnzao kapena kugonana ndi munthu wina amene si mwamuna kapena mkazi wao . ( 2 ) “ Zinthu zenizeni , ngakhale kuti n’zosaoneka . ” Amuna apaudindo afunika kukondwela pamene acinyamata amene iwo anawaphunzitsa bwino atenga maudindo . Nanga n’ciani cidzacitikila mabungwe ena onse oipa ? Ndinadziŵa kuti dzina la Mulungu ndi Yehova . Nifuna kuphunzila Baibulo . ” Akhristu onse atatu amenewa anasintha makhalidwe awo cifukwa cofunitsitsa kutengela Khristu . Mbali yoyamba inakwanilitsidwa pamene ulamulilo wa Mfumu Nebukadinezara unasokonezedwa . Panthawi ina iwo akali m’dziko la Harana , Yehova anakambanso na Abulahamu , kumuuza kuti acoke m’dzikoli na kuyenda kudziko limene Yehova anali kudzamuonetsa . Pulofesa wa zamalamulo dzina lake Alastair Kerr anafotokoza kuti mu 533 C.E . , Mfumu ya Roma Justinian , inafalitsa kope yokamba za malamulo a Aroma amene akatswili a zamalamulo anapanga ( ca m’ma 100 - 250 C.E . ) . Ambili mwa mafanizo amenewo anawachula mu ulaliki wake wa pa phili , wolembedwa m’buku la m’Baibulo la Mateyu macaputala 5 mpaka 7 . Muyenelanso kuwaganizila ofalitsa amene amalephela kucita zambili cifukwa ca kufooka kwa thanzi kapena pa zifukwa zina . Komanso , sitingalamulile anthu pa zocita zawo , aliyense ali na ufulu wake . ( 1 Maf . Mu 1879 , magazini yoyamba ya The Watch Tower inasindikizidwa mu Cingelezi . ( Pitani polemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACINYAMATA ) Monga mmene taphunzilila , njila yaikulu yoonetsela cikondi cimeneci ndi mwa kuuzako anzathu uthenga wa Ufumu . Mukakumana ndi mavuto aakulu , kapena ngati anthu ena anakucitilani zinthu zopanda cilungamo , ndipo vutolo likupitilizabe , musataye mtima . Kodi adani amphamvu amenewa tingakwanitse kuwagonjetsa ? Kodi tiyenela kumuona bwanji Yesu masiku ano ? Mu 1964 Mboni zinazunzidwa koopsa cifukwa cokana kutengako mbali m’ndale . Mosiyana ndi zimenezi , cimwemwe ni khalidwe lokhazikika la mu mtima . 15 MAFUNSO OCOKELA KWA AŴELENGI . . . Kungokhala amvetseli abwino kwakhala kothandiza kwambili . ” Ndi oopsa cifukwa amasoceletsa munthu pang’ono - pang’ono , koma iye osadziŵa . Mauthenga osoceletsa ali monga mpweya wakupha , koma wopanda fungo . N’zolimbikitsa kwambili kudziŵa kuti Mlengi wathu ndiponso ‘ mmisili wake waluso ’ ali ndi mphamvu zosayelekezeka . Mofananamo , abale na alongo amene amalakalaka kukhala apainiya , atumiki a pa Beteli , kapena kudzipeleka kumanga Nyumba za Ufumu , angacite bwino kupita patsogolo kuti akwanilitse zolinga zawo . Kristu wapatsa atumiki ake udindo wolalikila umene ndi wamtengo wapatali ( Onani ndime 10 ) “ Mvelani kuno nonsenu , ndipo mumvetse tanthauzo lake . ” — MALIKO 7 : 14 . 39 : 6 , 7 ) Komabe , Mulungu anali kuyembekezela nthawi imene adzaombola anthu ake amene adzalapa ndi kubwelela kwa iye . Patapita nthawi yocepa , mu December 1945 , gulu la Mboni za Yehova locokela m’tauni ya Angat linabwela kudzalalikila m’mudzi wathu . Masomphenya a namba 6 na 7 adzatithandiza kuyamikila mwayi wathu wotumikila m’gulu loyela la Mulungu . Komabe , pa 1 Yohane 5 : 7 , anawonjezelapo mawu olakwika amene tawachula kale m’nkhani ino . Iwo anagwilitsila nchito nthawi yaitali ya moyo wao ndi anchito ao masauzande ambili poyesa - yesa kulimbana ndi imfa . ( Num . 30 : 2 ) Pambuyo pake , Solomo anauzilidwa kulemba kuti : “ Ukalonjeza kwa Mulungu usamacedwe kukwanilitsa lonjezo lako , cifukwa palibe amene amasangalala ndi anthu opusa . 25 : 13 . ( b ) N’zinthu ziti zimene ise tifunika kusamala nazo masiku ano ? Ngakhale kuti Yehova ndi Wamkulu Koposa , akutipempha kuti tizipemphela kwa iye ndipo akutitsimikizila kuti adzamvetsela mapemphelo athu . A Pyarelal , omwe anali kalembela wa Malemu Mohandas Gandhi , mtsogoleli wacipembedzo ku India , anakamba kuti , a Gandhi anali kuona kuti : “ Dziko lapansi lili ndi zinthu zimene zingakwanitse kukhutilitsa zosoŵa zonse za anthu , koma osati kukhutilitsa zikhumbo zadyela za anthu . ” ( Gen . 1 : 28 ) Ngakhale kuti anawo akanakonda makolo awo , akanafunikila kucoka kuti akayambe mabanja awo - awo . Ningacite ciani kuti nipeze mabwenzi abwino na kukhala bwenzi labwino ? Ndipo anthu amene amakonda Yehova adzakhala osangalala kwamuyaya . Sikutanthauza kucepetsa colakwaco , kulekelela , kapena kunyalanyaza monga kuti sicinacitike . 6 : 3 , 4 ; Afil . Cosankha ni canu ! N’ciani cinathandiza Mose kuopa Yehova osati Farao ? Onani nkhani yakuti “ Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi — Kodi Akhristu Ayenela Kukondwelela Khrisimasi ? ” Yehova amafuna kuti muzipanga zosankha mwanzelu zokhudza tsogolo lanu . Motelo , tifunika kupitilizabe kukhala pakati pao ndi kugwilizana kwambili ndi mipingo yathu . Baibulo limatitsimikizila kuti Mulungu wakhala akugwila nchito kuti apulumutse anthu ake okhulupilika ndi kuti colinga cake cokhudza dziko lapansi cidzakwanilitsidwa . Nthawi zina ndinali kuwauza kuti ndinali kuphunzila Baibulo ndi kuti ndinali kufuna kukhala nzika yabwino . Conco n’zosadabwitsa kuti anathandiza Yosefe kudziŵa tanthauzo la maloto amene amuna anzelu ndi ansembe analephela kumasulila . Ndi gulu liti limene linaloŵa m’malo Aisiraeli ampatuko ? Masiku ano , tili na cifukwa comveka cokhulupilila kuti ‘ tsiku la Yehova lalikulu ndi locititsa mantha ’ lili pafupi . ( Yow . Tikadwala , tikataya mtima , tikakhala ndi cisoni , tikasauka , kapena tikakumana ndi mavuto ena , tiyenela kukhala ndi cikhulupililo cakuti Yehova ndi Yesu adzatithandiza “ pa nthawi imene tikufunika thandizo . ” Kodi tikudziŵa bwanji kuti a “ nkhosa zina ” adzasangalala pamodzi ndi banja lonse la Yehova pa cikwati ca Mwanawankhosa ? ( a ) Ni malangizo ati amene angatithandize kupanga zosankha mwanzelu ? M’nkhani ino , tiphunzila cifukwa cake tiyenela kuthetsa mikangano kapena kusamvana , ndi mmene tingacitile zimenezo . Yehova amatitsimikizila kuti “ aliyense wofuna kudalitsidwa padziko lapansi adzadalitsidwa ndi Mulungu wokhulupilika . ” Kodi acicepele angapindule bwanji ngati aseŵenzetsa malangizo apa Miyambo 16 : 3 ? Mulungu anaika Amosi kukhala mneneli wake . Ndithudi , uwu unali utumiki wapadela kwambili . Tikhulupilila kuti Mulungu , amene “ amaona mmene mtima ulili , ” adzakulitsa coonadi m’mitima ya anthu a maganizo oyenela . — 1 Sam . Zovala zathu siziyenela kupangitsa anthu kukaikila ngati ndife Mboni za Yehova . Tingayambe kuona ubwenzi wathu ndi iye mopepuka . Kodi kuganizila zimene zinacitikila Yosefe kungatithandize bwanji ngati Mkhristu mnzathu waticitila zinthu zopanda cilungamo ? Mu May 1971 , ndinafunika kupita ku Michigan kukasamalila mbali zina zofunika . ( Mat . 19 : 5 , 6 , 9 ) Inde , anthu a m’cikwati angacilikize ulamulilo wolungama wa Yehova mwa kucita zonse zimene angathe kuti alimbitse cikwati cawo . 4 : 16 . Koma zimene io anacita ndi kukamba ziyenela kuti zinam’dabwitsa kwambili . Abulahamu ndi Sara anaonetsa bwanji cikhulupililo cao mwa Yehova ? N’zoona kuti pambuyo pake n’namukhululukila , koma nimadziimba mlandu kuti n’nacedwa kucita zimenezo . Mwacionekele ndi Ufumu wa Mulungu wokha umene udzakhalapo mpaka kalekale osati boma lililonse la anthu . Si conco ? Kodi cikhulupililo cingakuthandizeni bwanji kupilila ngati zimenezi zakucitikilani ? Ndipo tikadwala , sitiyembekezela kuti Yehova aticilitsa mozizwitsa . Ndiyeno , kumapeto kwa zaka za m’ma 1800 , zinali ngati kuti mnofu ndi khungu zayamba kukuta mafupa . Amatithandiza kupitila mwa abale athu , akulu , kapolo wokhulupilika , angelo , ndi Yesu . Si anthu amene anapanga makonzedwe akuti pakhale mizinda yothaŵilako . 17 Kodi Mavalidwe Anu Amalemekeza Mulungu ? “ Zimenezo uziphunzitse kwa anthu [ amuna ] okhulupilika amene nawonso , adzakhala oyenelela bwino kuphunzitsa ena . ” — 2 TIM . ( Onani palagilafu 11 , 12 ) Mu 2014 , pambuyo pa zaka 2,000 , ku Turkey kunacitikanso nchito yapadela yolalikila . Iye anayankha kuti : “ Zimenezi n’zocititsa manyazi ndithu , koma munithandize . ” 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani sitiyenela kudabwa tikakhala na nkhawa ? Akakhala mumzindawo , anali kutetezedwa na Yehova . Ni zinthu zinayi izi : Amene anatipatsa , cifukwa cimene anatipatsila , zimene anatailapo kuti atipatse , ndiponso zosoŵa zimene inakwanilitsa . N’cifukwa ciani tiyenela kudziyesa kuti tione ‘ ngati tikali olimba m’cikhulupililo ? ’ Baibulo lingatithandize kupitiliza kusintha umunthu wathu kuti titengele Mulungu . Mwacitsanzo , angatithandize posankha nyimbo yoimba pa nkhani ya anthu onse . Kodi acikulile , acinyamata , ndi akazi awo , angacite ciani kuti asungitse mtendele ndi mgwilizano m’gulu la Yehova ? ( Yobu 31 : 1 ) Ngakhale pamene tikupumula kapena kusangalala kumbali kwa nyanja , kapena ponyaya mu swiming’ipuu , zovala zathu zonyaila ziyenela kukhala zaulemu . ( Deuteronomo 1 : 16 ) Oweluza angapeleke cigamulo cabwino pokhapo akakhala ndi umboni wonse wokhudza mlanduwo . Komabe , madzi oundanawo akapitiliza kusungunuka cifukwa ca kutentha , madzi a pansi pa nyanjayo pang’onopang’ono adzayamba kuonekela . 17 Kodi N’kumupatsilanji Amene Zonse N’zake ? AMENE AKUCITITSA MAVUTO AMBILI Tingathandize bwanji kuti m’nyumba ya Yehova musakhale zoipa zilizonse ? Paulo anafotokoza kuti : “ Zinacita kulembedwa kuti : ‘ Munthu woyambilila , Adamu , anakhala munthu wamoyo . ’ Anadziŵa kuti Yehova sakonda anthu amene amasungila anzao cakukhosi ndiponso amene amabwezela . Ndipo iye anafuna kutengelapo mwai wakuti awaphunzitse coonadi ca mtengo wapatali . ( Mlal . 8 : 16 , 17 ) Kudalila Yehova kudzatithandiza kuzindikila ndi kuvomeleza , kuti sitingakwanitse kucita zonse zimene tifuna . Kungochulako ocepa cabe , m’banja na mu mpingo mumakhala mtendele . Anacita zimenezi kuti anthuwo afunefune Mulungu , amufufuzefufuze ndi kumupezadi , ngakhale kuti kwenikweni , iye sali kutali ndi aliyense wa ife . ” ( Mac . ( Tito 2 : 12 ) Kakambidwe kathu , kadyedwe ndi kamwedwe , kavalidwe na kudzikonza kwathu , ngakhale mmene timaseŵenzela ku nchito , zonse ziyenela kuonetsa kuti ndise anthu odzipatulila kwa Yehova . — Ŵelengani 1 Akorinto 10 : 31 , 32 . Zimenezi n’zolimbikitsa kwambili cifukwa zionetsa kuti Yesu adzacita zinthu zambili m’dziko latsopano . NYIMBO : 128 , 45 ( Yoh . 13 : 12 - 17 ) Tifunikanso kumapempha mzimu wa Mulungu kaŵili - kaŵili kuti uzitithandiza kupewa mzimu wodziona ngati ndise wofunika kwambili kuposa anthu ena . — Agal . ( Aheberi 11 : 32 , 33 ) Yehova anayankha mwa kulola Debora kupitila limodzi ndi Baraki . Tifunika ‘ kuyesetsa mwakhama , ’ kapena kuti kugwililapo nchito . Mkate weniweni unali cakudya ca tsiku ndi tsiku ca Ayuda monga mmene mana analili cakudya ca Aisiraeli kwa zaka 40 m’cipululu . M’mapikomo , ndi mmenenso anapiye ake amabisalila mvula yamphamvu ndi dzuwa . Iye anagwilanso mau a mu kalata ya Agiripa Woyamba , mdzukulu wa Herode Wamkulu , yopita kwa Mfumu Yaciroma dzina lake Kaligula . Zimenezi zikutanthauza kuti tifunika kucitanso zina kuonjezela pa kuphunzila mfundo ndi malamulo a Mulungu . ( Genesis 40 : 8 ) Mau amene Yosefe anakamba ndi othandizanso masiku ano kwa anthu onse okonda kuphunzila Baibulo . * ( 1 Mafumu 21 : 5 - 14 ; Levitiko 24 : 16 ; 2 Mafumu 9 : 26 ) Ahabu ananyala - nyaza udindo wake monga mutu wa banja ndi kutsatila zofuna za mkazi wake za kupha anthu osalakwa . Ambili m’kilasi mwake anali na khalidwe laciwelewele cakuti akabwela kusukulu pa Mande , anali kucita kukamba monyadila za anthu amene anagona nawo kumapeto kwa wiki . Kungakhale kupanda nzelu ndiponso kulakwa kusiya Yehova ndi anthu ake cifukwa cakuti munthu winawake watilakwila ( b ) Kodi tingapewe bwanji citsanzo coipa ca Sauli ? Kodi cinthu coyamba cimene Mfumu yatsopano inacita cinali ciani ? Nanga kodi inacita ciani pambuyo pake ? ( Ŵelengani Aheberi 12 : 3 . ) Alan akukumbukila mau a Yesu akuti : “ Zimene mukufuna kuti anthu akucitileni , inuyo muwacitile zomwezo . ” Anawo ayenela kudziŵitsa akulu a ku mpingo wa makolo ao ponena za cisamalilo cimene banja lingapeleke . Ndinayamba kuona mkazi wanga moyenelela . Komanso , timayamikila kuti Mulungu anatipatsa moyo , umene timatha kusangalala nawo . 30 Mphamvu ya Moni Kwa kanthawi , iye anaiŵala mmene Yehova anam’thandizila m’mbuyomo . ( Mateyu 16 : 8 ) Komabe , pali phunzilo lofunika kwambili pa cocitika ca Petulo . 115 : 1 . M’malo mopemphanso thandizo kwa Yehova , iye anacita pangano ndi mitundu yakunja . Koma Yehova anam’patsa dzina lakuti Abulahamu , limene limatanthauza “ Tate wa mitundu yambili . ” Mwacitsanzo , pa nthawi ina anthu a ku Galileya anapita kukamufunafuna . Kuti mumve zambili zokhudza cizunzo ca ku Malawi , onani Buku Lapacaka la Mboni za Yehova la mu 1999 , patsamba 171 mpaka 223 . Kodi lemba la Salimo 41 : 3 lingatilimbikitse bwanji tikadwala ? Tsiku lina mlonda amene anali kutiyang’anila m’munda umene tinali kulima anadwala , ndipo tinamunyamula ndi kubwelela naye kundende kuti akalandile thandizo . M’nkhani ino , tikambilana mmene alongo amaonela nkhaniyi , koma mfundo zake zikhudzanso abale . Iye anati : “ Pemphela kwa Atate wako . ” Kodi mukanakhala inu mukanacita ciani mutamva lonjezo la Yehova Mulungu limeneli ? Davide anakana kubwezela coipa kwa Sauli ngakhale pamene mpata unapezeka wocita zimenezo . ( Dan . 9 : 1 , 2 ) Danieli anali kum’dziŵa bwino Mulungu , kuphatikizapo mmene anali kucitila zinthu ndi Aisiraeli . Umboni wa zimenezi ni pemphelo lake lolapa locokela pansi pa mtima , lolembedwa pa Danieli 9 : 3 - 19 . Popeza kuti anali wangwilo , mosakaikila iye anali “ wokongola . ” Tiyenela kuziseŵenzetsa pa kulemekeza Mulungu na kuthandiza anthu ena . Koma sicinali copepuka kwa iwo pa zifukwa zingapo . Satilamula kucita zinthu zimene sitingakwanitse . Koma nthawi zonse , amatilamula kucita zimene tingakwanitse . Iye amaona kuti magazi amaimila moyo . ( Gen . N’ciani cimene tingakambe kuti tilimbikitse a mtima wacisoni ? Uphungu wa m’Baibo ungatithandize kupewa mavuto Tiyeni tisangalale ndipo tikhale ndi cimwemwe codzaza tsaya . Timupatse ulemelelo , cifukwa ukwati wa Mwanawankhosa wafika , ndipo mkazi wake wadzikongoletsa . ” — Chiv . Cifukwa nthawi zambili kucita zimenezi kumawabweletsela cimwemwe . ( Sal . Tidzasangalala kwambili pamene anthu sadzaphedwanso kapena kuvulala ndi ngozi zacilengedwe , cifukwa cakuti “ cihema ca Mulungu [ cidzakhala ] pakati pa anthu . ” ( Chiv . Pali makhalidwe ambili ofunika , koma otsatilawa ni othandiza kwambili : Ponena za “ olandila coloŵa anzake a Kristu , ” mtumwi Petulo anati : “ Inu ndinu ‘ fuko losankhidwa mwapadela , ansembe acifumu , mtundu woyela , anthu odzakhala cuma capadela , kuti mulengeze makhalidwe abwino kwambili ’ a amene anakuitanani kucoka mu mdima kuloŵa m’kuwala kwake kodabwitsa . ” ( 1 Pet . ( Salimo 91 : 11 ) Mngelo mmodzi anapha asilikali 185,000 a Asuri usiku umodzi ndi kupulumutsa anthu a Mulungu . Koma tidzacita zilizonse zimene tingathe kuti ‘ ticitile umboni mokwanila za uthenga wabwino . ’ ( Mac . 20 : 24 ; 2 Tim . Koma ngati m’kupita kwa nthawi makolo ayamba kuvutika kuyenda , kugula zinthu zofunikila , kapena kuiŵala - iŵala , ana angafunikile kusintha zinthu zina . Nthawi zina pambuyo pokambilana , tingazindikile kuti mnzathuyo sanaticitile zinthu zopanda cilungamo . Munthu akaphunzila za Yehova ndi kubatizidwa , amapitiliza kukulitsa ubwenzi wake ndi Mulungu . Kodi anyamata anai aciheberi amene anali ku Babulo anaonetsa bwanji kuyamikila coonadi cimene anaphunzila ? Colinga ca Yehova Cidzakwanilitsika , Feb . N’ciani cina cinawathandiza ? Kodi akanalela mwana wake ‘ m’malangizo a Yehova ndi kum’phunzitsa kaganizidwe kake ’ pa Intaneti ? — Aef . Mwa njila imeneyo mudzamuthandiza kugwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo . pa www.jw.org Sangalephele kucita ciliconse kapena kupangitsa ciliconse kucitika kuti akwanilitse cifunilo cake Kodi Arthur anali na mpeni ? Tsopano ophunzila a Yesu anafunikila kudziŵitsa anthu colinga ca Yehova catsopano . Colingaco cinali cofunika kwambili kuposa kumasulidwa kwa Aisiraeli ku ukapolo ku Iguputo , ndiponso pambuyo pake ku Babulo . Webusaiti imeneyi idzakuthandizani kudziŵa zambili zokhudza Baibulo kwaulele m’zinenelo zoposa 700 . N’natsimikiza Mtima Kukhala Msilikali wa Khristu ( D . Kodi mungakonde kudziŵa zambili za madalitso amenewa ? 2 : 5 . Komabe , tifunika kuyembekezelabe ngakhale kuti tacita zimenezo kwa nthawi yaitali . Mwacitsanzo , ngati tinawalemba nchito , timacita nao zinthu mwacilungamo ndi kuwapatsa malipilo mogwilizana ndi zimene tinapangana . Ni mfundo ziti zimene zionetsa kuti Mkhristu sayenela kukhala na mfuti yodzitetezela kwa anthu ena ? Anthu ena asanakhale Mboni anali na zizoloŵezi zoipa monga kudya kwambili , kumwa kwambili , kupepa fwaka , kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza ubongo , ciwelewele , ndi zina . Ndinaganiza zoyamba upainiya , ndipo ndinayamba kupemphela kwa Yehova tsiku lililonse kuti andithandize kukonda ulaliki . ” Aiguputo anapanga anthuwo kukhala akapolo okumba migodi , kumanga akacisi , na kukumba mifolo ya madzi . M’malo mwake , zingakhale zosavuta ‘ kutengeka ndi nkhawa , cuma ndi zosangalatsa za moyo uno . ’ — Luka 8 : 14 , 15 . Komanso anthu anali kumukonda kwambili cifukwa ca cikondi ndi kudzicepetsa kwake . Anali kumukondanso cifukwa cotsatila malamulo ndi mfundo zolungama ndiponso cifukwa cokhulupilila kwambili Yehova . N’zosangalatsa kwambili kugaŵila zofalitsa zokongola ndiponso zothandiza zimenezi mu utumiki . ( Aroma 8 : 16 , 17 ) Anthu amene adzakhala padziko lapansi akuyembekezela moyo wosatha . Kuti nikafike ku matauni ena , n’nali kupitila m’mapili a miyala ochedwa Sierra Madre . Ali wacinyamata , Mose anali ndi mwai wokhala m’nyumba yacifumu pamene Aheberi ena anali akapolo . 14 : 9 ) Yesu anatengela kwambili umunthu wa Atate wake cakuti tikamaphunzila za iye timakhala ngati tikuphunzila za Yehova . Mwacitsanzo , Afarisi anali kuona ophunzila a Yesu kuti anali m’gulu la anthu “ otembeleledwa . ” Dzina lake limatanthauza kuti “ Amacititsa kukhala . ” Pa zaka zoposa 10 zapitazi , ciŵelengelo ca apainiya cinafika 13,224 mu October 2015 . Asanaphunzile coonadi , ena mwa abale na alongo athu anali kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza ubongo , kuba , ndi kucita ciwelewele . ( Mateyu 5 : 3 ) Anapeza mabwenzi abwino pakati pa okhulupilila anzake . Yehova amakondwela kwambili ndi kupeleka mphoto . ( Ŵelengani Chivumbulutso 7 : 12 . ) Komanso , ena angakhale na nkhawa kwambili pambuyo powapeza na matenda aakulu , kapena angakhale na cisoni cacikulu cifukwa ca imfa ya munthu amene anali kum’konda . Sitingaleke kugwilitsila nchito moto cifukwa coopa kuti utishoka . Pamene tikuyandikila mapeto a dzikoli , maboma ambili adzayamba kutikakamiza kutenga mbali m’zandale . Ise tifunika kukhala osamala kwambili , mwina kuposanso Aisiraeli . Pamene anafuna uphungu wa mmene angayendetsele ufumu wake , coyamba anakafunsila kwa acikulile . Inunso mungakhale wokhulupilika kwa Yehova ndi kwa ena mwa kukhala wokoma mtima . Zimenezi zimacititsa kuti afune kucita zambili . ” Kuti ndilalikile asodzi ambili , ndimaphunzila ndi anthu anai kapena asanu panthawi imodzi . ” Zida monga Watch Tower Publications Index kapena Buku Lofufuzila Nkhani la Mboni za Yehova , zingakuthandizeni kupeza zofalitsa zofotokoza nkhani zosiyana - siyana , ndi zina zofotokoza mavesi ambili a m’Baibo . Ngati tayatsa moto , umakhala wamphamvu kwambili . Timoteyo anaona kuti Paulo anali kutsatila mau amenewa paumoyo wake . 9 : 36 - 42 . Mwiniwake bwatolo anali cheyamani wacipani m’delalo . Tidzakambilana ciani m’nkhani ino ? Ndinatsimikizila kuti abale amene ndinali kuphunzitsa anamvetsetsa malangizowo . ( Mat . 24 : 3 , 7 - 14 ) Popeza Yesu sanakambe utali wa nthawi ya mapeto imeneyi , tifunika kukhalabe maso . 16 : 23 , 24 ) Masana a tsiku limenelo , gulu la anthu aciwawa linawagwila mwadzidzidzi ndi kuwakokela kumsika kuti akaime pa bwalo la oweluza . Kodi nimaona kuti kufuna - funa ndalama ndiye cinthu cofunika kwambili ? Ganizilani mmene boma la padziko lonse lingathandizile anthu . Cifukwa cakuti tinali kulephela kudya ndipo tinali okhudzika kwambili , io anatitenga kukakhala nao kwa kanthawi . ” Mkazi wanga Maria anaphunzila coonadi ku Ukraine mkati mwa Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse . Cilumba ca Simeulue cinali coyamba kuonongedwa ndi tsunami wa pa Nyanja ya India . Aisiraeli akamvela Mulungu , iye anali kuwadalitsa . Mu 1969 , M’bale wina dzina lake Angelo Manera atafika ku msonkhano ku Dodger Stadium mumzinda wa Los Angeles , ku California , anauzidwa kuti waikidwa kukhala mtumiki wa kafiteliya . Ngakhale ndi telo , iye anavomela kuti tikwatilane , ndipo titakwatilana tinayamba kukhala kumudzi ngakhale kuti iye anakulila ku tauni . Kaŵili - kaŵili anthu a khalidwe lonyada saimvetsetsa Baibo , ndipo khalidwe limeneli n’lofala pakati pa anthu “ anzelu ndi ozama m’maphunzilo . ” ( b ) N’colinga ca Yehova catsopano citi cimene ophunzila a Yesu anadziŵitsa anthu ? 5 : 28 ) Kupewa kucita zimenezi kungakhale kovuta . Koma tifunika kuyesetsabe kuti Yehova atidalitse . ‘ Tinamasulidwa ku ucimo ’ ndi ‘ kukhala akapolo a cilungamo . ’ ( Mateyu 22 : 39 ) Timadziŵa kuti anthu ambili ali ndi zipembedzo zao ndipo timadziwanso kuti si anthu onse amene angalandile uthenga wathu . Iwo sayenela kucita cinthu ciliconse cokhudzana ndi kulambila mafano . ( a ) Kodi cofunika kwambili n’ciani kuti tikapeze moyo wosatha ? Anasinkha - sinkha lemba limene linafotokozedwa pa umodzi mwa misonkhano yathu , ndipo anagwilizanitsa mfundo ya pa lembalo na malemba ena . Iwo amalimbikitsidwa kwambili ngati abale ndi alongo awathandiza pa zosoŵa zao ndi kuonetsa kuti amawakonda . 5 : 1 - 4 ) Kukumbukila kuti “ Mulungu adzaweluza adama ndi acigololo , ” kumathandiza okwatilana kucita khama kuti cikwati cao cikhale colemekezeka ndi cosaipitsidwa . — Aheb . Iye analeledwa m’banja lacifumu la Aiguputo , pamene Iguputo unali ulamulilo wamphamvu koposa padziko lonse . Koma ngati mwamuna ndi mkazi amakhululukilana potengela citsanzo ca Yehova , banja lao limakhala lolimba . — Mika 7 : 18 , 19 . Iye anapita kunyumba “ ali wacisoni ndi wokhumudwa ” cifukwa cakuti zofuna zake sizinacitike . Kuuzako ena uthenga wabwino kumanipatsa cimwemwe Baibulo limatitsimikizila kuti : “ Buku la cikumbutso linayamba kulembedwa pamaso pake . Buku limeneli linali lonena za anthu oopa Yehova ndi anthu amene anali kuganizila za dzina lake . ” — Malaki 3 : 16 . Mungapeleke zopeleka zanu m’njila izi : Kucita zimenezi kumathandiza kuti mumpingo mukhale bata ndi mtendele . — Mac . 6 : 1 - 4 . Mwina mwakumbukila mau ena a m’citundu canu amene muona kuti asintha kwambili tanthauzo . Kukali zaka 30 , mngelo Gabirieli anauzilatu Mariya kuti : “ Udzakhala ndi pakati ndipo udzabeleka mwana wamwamuna , . . Cifukwa cakuti simungadziŵe mavuto amene mudzakumana nawo mtsogolo . Mwacitsanzo , kunyada kapena umbombo , zingaticititse kuti ticite chimo lalikulu . Popeza Yesu Kristu ndi Mfumu ya Ufumu wa Mulungu wa kumwamba , posacedwapa adzacotsa zoipa zonse padziko lapansi . Ndipo adzasandutsa dziko kukhala paladaiso kuti anthu akakhalemo kwamuyaya . Onse amene anapezekapo anasangalala kwambili . Conco , n’naleka kuzitsatila . Mwacitsanzo , Kaini anapha m’bale wake Abele cifukwa ca nsanje . Wina anali Oswald Schreckenfuchs , katswili wa ku German wa m’zaka za m’ma 1565 . Kodi kukhulupilila Mulungu kuli ndi phindu lotani ? N’cifukwa ciani ndimakhulupilila kuti miyezo ya Yehova ingandipindulitse ? ” Komabe , kumbukilani kuti : Kucita zinthu za kuuzimu nthawi zonse kungakuthandizeni kulimbana ndi mayeselo aakulu mtsogolo . 24 : 21 ) Ndipo m’malo moonetsa kuwala kwambili kwa anthu a m’dela lathu , kuwala kwathu kudzayamba kuzimililika kapena kudzazimilatu . Kuyambila ali ana , io anali kutumikila mumpingo umodzi cabe . Ndipo anali kukhala pafupi ndi acibale ao ambili . Pamene anali kukula , nthawi zina anali kudandaula cifukwa cocita phunzilo la banja . Patapita nthawi , Petulo anachula makhalidwe amene tiyenela kukulitsa . ( Yesaya 29 : 13 ) Mtunduwo utalephela kusintha , Mulungu analola olamulila amphamvu kuti aononge Yerusalemu ndi kacisi wake , likulu la cipembedzo ca Aisiraeli . Ungachulenso mfundo zothandiza za m’Baibulo , monga zopezeka mu Ulaliki wa pa Phili . Okwatilana angalimbitse ukwati wao mwa kulankhulana bwino ( Onani ndime 15 ) Yesu Kristu atakhala Mfumu yatsopano , anayamba kulanditsa otsatila ake odzozedwa kucoka mu ukapolo ku “ Babulo Wamkulu . ” Kodi inu muli pabanja ? 3 : 7 ) Kodi Yehova anapeleka bwanji “ mphatso yaulele ” imeneyi ? Nanga n’cifukwa ciani ? 5 : 9 ) Koma kodi n’ciani cimatipangitsa kukhala osiyana kwambili ndi gulu lina lililonse la anthu ? Conco , pamene makolo acikhristu akuphunzitsa ana awo kuyambila ali aang’ono , afunika kukhala na colinga cowathandiza kukhala ophunzila a Khristu obatizika . ( Luka 10 : 3 , 5 , 6 ) Anthu ena amene timakumana nawo mu ulaliki amakhala aukali kapena acipongwe . Citsanzo 1 : Tikakumana ndi munthu mu ulaliki amene amakhulupilila kuti Yesu ndi wolingana ndi Mulungu . Conco , tipitilize kucitila umboni mwakhama ndi kukhalabe oyela m’dziko lodetsedwa la Satana . Kodi nimakhulupililadi kuti Yehova adzanipatsa zosowa zanga ? ’ buku la Yesaya Mlungu uliwonse amagwilizana ndi ofalitsa amene amalalikila kudooko lalikulu la ku Taiwan . Koma pemphelo lamuthandiza kwambili . Apolisiwo anakondwela kumva zimenezo cakuti anachela tepi kuti ajambule mau anga . Ngati muyesetsa kukhomeleza coonadi ca m’Baibo m’mitima ya ana anu , Yehova adzakudalitsani kwambili . — Sal . Imwe acicepele , ngati umu ni mmene zinthu zilili mu umoyo wanu , mungacite bwino kuganizila citsanzo ca Mose . Mosiyana ndi Mfumu Davide , Rehobowamu analephela kupanga ubwenzi wabwino na Yehova 1 : 24 ; 1 Ates . 5 : 12 , 13 ) Iwo amafunitsitsa kugwila nchito mwakhama ndi kutsatila malangizo . Zaka 7 zapitazo , William ndi Jennifer a ku United States , anasamukila ku Taiwan . “ Kulambila kwa pabanja kumatipatsa mpata wolankhula maganizo athu momasuka . Nthawi zina ndi bwino kukhala cete . Mosiyana ndi zimenezi , ife Akristu timalimbikitsidwa tikamaganizila za ciyembekezo cathu , kaya ndi ca kumwamba kapena ca padziko lapansi . Mboni za Yehova zimakhulupilila kuti “ Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu , ndipo ndi opindulitsa . ” “ Tiyeni tisangalale ndipo tikhale ndi cimwemwe codzaza tsaya . . . cifukwa ukwati wa Mwanawankhosa wafika . ” — CHIV . Nanga kodi kukhala munthu wauzimu kungakhudze bwanji umoyo wathu wa tsiku na tsiku ? Acicepele — “ Pitilizani Kukonza Cipulumutso Canu , ” Dec . Abale na alongo pafupi - fupi 550 okamba citundu ca Citeki , anapita kudziko la Turkey kuti akagwile nchito yapadela imeneyi pamodzi na ofalitsa a kumeneko . Koma Mulungu anaona kuti afunika kum’thandiza Yobu kuwongolela maganizo ake . Pambuyo pa mwambo wa cikwati cimeneci , Kristu ndi mafumu anzake adzadalitsa kwambili anthu okhala padziko lapansi . — Chiv . Akhristu onse amene ali na udindo wopeleka cilango ca m’Malemba , afunika kutengela citsanzo ca Khristu . Ma Baibo ena amamasulila mau amenewa kuti , “ odana ndi zabwino ” kapena kuti “ oipidwa na ciliconse cabwino . ” 4 : 1 , 2 . ( Ŵelengani Yeremiya 31 : 31 - 33 . ) Ngati tisinkhasinkha zimene Baibulo limakamba , timayamba kuona zinthu mmene Mulungu amazionela . 14 , 15 . ( a ) Kodi anthu anali kuwaona bwanji Akristu m’nthawi ya atumwi ? Nanga mtumwi Petulo anati ciani ponena za io ? Musamaŵelenge mothamanga Kodi tiphunzilapo ciani pa mau amenewa ? Ndi phunzilo lotani limene titengapo pa fanizo la Paulo la “ cidindo ” ? Kodi mkwatibwi akumubweletsa kwa “ mfumu ” iti ? Nanga mkwatibwi ameneyo wavala zovala zotani ? M’mbuyomo , iwo ananipatsako magazini a Nsanja ya Mlonda na Galamukani ! Cifukwa Mau a Mulungu amaletsa ciwelewele . ( 2 Akorinto 9 : 7 ) Kodi tikakhala owolowa manja ndani amapindula ? Kwanithandizanso kuti nikwanitse kupilila mavuto amene nimakumana nawo tsiku na tsiku , ” anatelo mlongo wina wa ku Canada . Tsiku lina Peter anafunsa Don kuti : “ Kodi iwe uvutikilanji na ine ? Yehova ndi “ Wakumva pemphelo , ” ndipo amathandiza onse omufunafuna mwa cikhulupililo . Conco , tinganene kuti Rakele anali monga cizindikilo ca amai onse a mtundu wa Isiraeli , a mu ufumu wa kumpoto ndi mu ufumu wa kumwela . 11 : 2 ; Chiv . 14 :⁠ 4 ) Apa n’zoonekelatu kuti Yesu anali kupeleka uphungu ndiponso cenjezo kwa otsatila ake odzozedwa pamene anali kufotokoza fanizo lopezeka pa Mateyu 25 : ​ 1 - 13 . Mlimi amagaula nthaka kuti nthakayo ikhale yofewa asanabyale mbeu . Ezekieli anatengewa kupita ku ukapolo mu 617 B.C.E . N’cifukwa ciani angamuone conco ? Yesu anali ataukitsapo anthu aŵili m’mbuyomo panthawi zosiyana . Ndipo munthu afunika kudzipeleka , kubatizika , na kupitiliza kutumikila Mulungu mokhulupilika kuti akakhale na mwayi woikiwa cizindikilo ca cipulumutso pa cisautso cacikulu cimene cikubwela . — Mat . John anati : “ Mosasamala kanthu za vuto langa , ndinali kuonetsetsa kuti ineyo ndi banja langa tikucita zinthu za kuuzimu nthawi zonse . “ Iwo sadzafanso . ” Muzikumbukila mmene munakhalila bwenzi la Yehova . Mau amenewa angatithandizenso kumuona moyenelela . Komabe , simungafunikile kumapeleka mphatso pa zocitika zapadela cabe . Kucipatala kumene ndinali kuseŵenza anali kundilipila pambuyo pa milungu iŵili iliyonse , ndipo ndalama zimene ndinalandila ndinali nditagulila zovala zoyendela mu ulaliki . 5 , 6 . ( a ) Kodi Yehova anamvela bwanji Yesu atabatizika ? Pokumbukila zimene anasankha , Serge aona kuti anasankha mwanzelu . Bukuli likupezekanso pa webusaiti yathu ya www.jw.org . ( Ŵelengani Luka 2 : 46 . ) Monga ophunzila Baibo , tinganene kuti Ufumu wa Mulungu unabwela m’caka ca 1914 pamene Yesu anaikidwa monga Mfumu kumwamba . Ciliconse cimene anapanga cimagwilizana ndi miyezo yake yapamwamba . ( Gen . ( b ) Nanga anthu amene sanali Aisiraeli anafunika kucita ciani kuti alambile Yehova ? Anthu a Yehova amadziŵika kwambili kuti amadzipeleka kuthandiza anthu panthawi ya masoka . Cikondi sicilimbikitsa munthu kucitila mnzake zoipa , cotelo cilamulo cimakwanilitsidwa m’cikondi . ” ( 1 Petulo 2 : 21 ; 1 Yohane 2 : 6 ) Timaonetsa kuti timakonda Mulungu ndi Kristu mwa kukhala womvela . 10 : 11 ; 15 : 12 , 13 ) Ndipo cifundo cimene Yesu anasonyeza cimaonetsa kuti Yehova amakonda mtumiki wake aliyense payekha . — Yoh . 5 : 19 . 8 : 31 , 32 ) Koma Satana safuna kuti tidziŵe coonadi . Amapita ku kacisi wamkulu wochedwa Ise kumene amalambila mulungu wamkazi wa dzuŵa wochedwa Amaterasu Omikami . Iwo akhala akulambila mulungu ameneyu kwa zaka 2,000 . Mtsikanayo anali kudziŵa kuti m’busayo anali kukonda Yehova komanso anali ndi makhalidwe abwino . “ Kodi mpheta ziŵili si paja amazigulitsa kakhobidi kamodzi kocepa mphamvu ? ( Salimo 139 : 14 ) Kodi sizimakucititsani mantha mukaganizila mmene mwana wakhanda amakulila kucokela ku selo limodzi ? MU November 2010 , mbiya inayake yakale kwambili ya m’dziko la China , anali kuitsatsa pa mtengo wa madola pafupifupi 70 miliyoni , ku England . NYIMBO : 86 , 54 Mwansanga iye anakapempha thandizo kwa akulu . Koma sanalinso woyenelela kukhala mpainiya kapena mtumiki wothandiza . Asayansi atulukila zinthu zambili kuthambo komanso pa dziko lapansi , ndipo agwilitsila nchito zinthuzo kuti umoyo ukhale wabwinoko . ( Zek . 13 : 4 - 6 ) Conco , zikuoneka kuti ngakhale atsogoleli ena a zipembedzo adzacoka m’zipembedzo zao ndi kuyamba kukana kuti anali m’zipembedzo zimenezo . Ena amanama kuti apewe kulandila cilango cifukwa ca macimo amene acita . CAKA ciliconse , anthu oposa 6 miliyoni amayenda ulendo wautali wopita ku thengo la cedar pacilumba cochedwa Shima ku Japan . Baibulo imaticenjeza kuti : “ Musalole kuti coipa cikugonjetseni , koma pitilizani kugonjetsa coipa mwa kucita cabwino . ” Kodi ndi mau ati amene si acilendo mu ulosiwu ? Tingacite ciani kuti mavuto a m’banja asakatimanitse mphoto ? Koma m’dzikoli anthu ni odzikonda , sakondanso abululu awo , ndipo kulimbitsana n’kosoŵa . Lemba la Yohane 17 : 3 limati : “ Pakuti moyo wosatha adzaupeza akamaphunzila ndi kudziŵa za inu , Mulungu yekhayo amene ali woona , ndi za Yesu Kristu , amene inu munamutuma . ” Patsiku lacitatu pamene Mariya Mmagadala ndi Mariya wina uja anabwela kudzaona manda , anapeza kuti mngelo wagubuduza cimwala ndipo wakhalapo . Yesu anali ndi zifukwa zomveka pamene anawauza kuti aleke kudela nkhawa . Mosiyana ndi Baibulo limeneli , palinso mabiliyoni a Mabaibulo ena athunthu kapena mbali yake m’zinenelo zina masauzande . Tiyeni tione zizindikilo zingapo . “ Ndi mwai wamtengo wapatali kuti Yehova akukamba nafe m’cinenelo cathu ” Adamu na Hava atangopanduka m’munda wa Edeni , Mulungu anapeleka ulosi wolimbikitsa umene unapatsa ciyembekezo mbadwa za Adamu zam’tsogolo . Koma m’maŵa mwa tsiku limenelo , John anadziceka kwambili pa cala pamene anali kutsegula lidi ya cithini . ‘ Mvelani ndi Kumvetsa Tanthauzo Lake , ’ 12 / 15 Baibulo limatilangiza kuti “ tiganizilane , ” kutanthauza kuti pamene tasonkhana pamodzi ndi abale ndi alongo athu , tiziganizila zosoŵa zao . ( 1 Akor . 7 : 39 ) Nanga n’cifukwa ciani angalankhule zofanana ndi zili pamwambazi ? Amene amakamba mau ngati amenewo amaona kuti pali alongo ambili kuposa abale . Ngati pacitika ngozi ya cilengedwe , acicepele amadzipeleka kuti agwile nchito pamodzi ndi abale ena yothandiza amene akhudzidwa . Wokwelapo wake ananyamula uta . Iye anapatsidwa cisoti cacifumu , ndi kupita kukagonjetsa adani ake ndipo anapambana pa nkhondo yolimbana nawo . ” — Chivumbulutso 6 : 2 . Kumbukilani kuti wopha mnzake mwangozi akakhala mumzinda wothaŵilako , sanali kukhalanso mwamantha poopa wobwezela magazi . Pamene Yesu anali kukamba zimene zidzaonetsa kuti tili m’masiku otsiliza , anafotokozela ophunzila ake mafanizo angapo . Tingacite zimenezi ngati zinthu zina zasintha . Kukhulupilika kwa Yosefe kunam’patsa mwayi woona mmene Yehova anakonzela zinthu zopanda cilungamo ndi kum’dalitsa pamodzi na banja lake . Koma m’maiko ena , mwakhalako nthawi za mtendele , ndipo panthawizi anthu a Yehova akhala akulalikila popanda zovuta . Sitiyenela kuwafunsa mmene anadzozedwela cifukwa iyi ndi nkhani yaumwini , ndipo sitifunika kudziŵa . ( Maliko 6 : 30 - 32 ) Lonjezo la Yesu lakuti adzaticilikiza likugwilabe nchito masiku ano . Mwacitsanzo , ganizilani za Hans , amene ni mkulu mumpingo wina ku Austria . Mungaŵelenge macaputala amenewo mwina kwa mphindi 15 kapena 20 , ndipo mudzadabwa ndi mau a Yesu osavuta koma amphamvu kwambili . ( 2 Sam . 16 : 16 ; 1 Mbiri 27 : 33 ) Iye ayenela kuti anali nduna ya panyumba ya mfumu komanso mnzake wa mfumuyo . Mphoto imene tidzalandila pocita zimenezi idzakhala yamuyaya , ndaŵa Paulo anati : “ Cifukwa malipilo a ucimo ndi imfa , koma mphatso imene Mulungu amapeleka ndi moyo wosatha kudzela mwa Khiristu Yesu Ambuye wathu . ” — Aroma 6 : 23 . Kodi panakhala zotulukapo zotani ? Kodi pali njila ina iliyonse imene tingadziŵile kaya imfa ndi mapeto a zonse ? Ndiponso , kumatipatsa mwayi wotumikila Yehova . Mpingo wacikhristu utakhazikitsidwa , kuimba nyimbo kunakhalabe mbali yofunika pa kulambila koona . 119 : 165 ; Aroma 8 : 37 - 39 . Ngati tiwatsatila , tidzaonetsa kuti timam’konda ndi kum’dalila . Conco , zikuoneka kuti makambilano a anamwaliwo akuonetsa zimene zidzacitike cisautso cacikulu cikatsala pang’ono kutha . 32 : 5 - 10 . Koma muyenela kukhala wosamala kuti musabatizidwe cabe cifukwa cakuti mwafika pa msinkhu winawake kapena cifukwa cakuti anzanu ambili akubatizidwa . “ Nkhosa ” zimenezo zikuyembekezela moyo wosatha padziko lapansi , umene Adamu ndi Hava akanakhala nao . 6 : 4 ) Cinanso , muziwapemphelela ndi kupemphela nawo pamodzi . Tom , amene wakhala mkulu kwa zaka zambili , anati : “ Mkulu wina amene watumikila nthawi itali anayamba kunionetsa cidwi , ndipo ananiphunzitsa zambili . Iye anayamba kugwilitsila nchito “ lupanga la mzimu , ” limene ni Mau a Mulungu , polalikila uthenga wamtendele kwa anthu a mtundu uliwonse . ( Aef . M’nkhani yotsatila tidzakambilana mmene ife tonse tingawathandizile kutumikila Yehova mokondwela . Mu 2010 , Sukulu Yophunzitsa Utumiki inayamba kuchedwa Sukulu Yophunzitsa Baibo ya Abale Osakwatila , ndipo panakhazikitsidwa sukulu yatsopano yochedwa Sukulu Yophunzitsa Baibo ya Akristu Ali Pabanja . Kodi ndimapeza bwanji zosowa zanga za kuthupi ? Yehova amafufuza mitima ya anthu kuti aone amene amam’konda . ( 2 Akorinto 9 : 7 ) Mu 1879 , magazini ya Nsanja ya Mlonda , imene panthawiyo inali kuchedwa Zion’s Watch Tower , inati : “ Sitikaikila kuti YEHOVA ndi amene akutsogolela nchito yofalitsa magazini ino , motelo sitidzapemphetsa kwa anthu kapena kuwacondelela kuti athandize pa nchito imeneyi . ” Mu 1967 , ndinayamba kuphunzila cinenelo cimeneci mumzinda wa Jena , umene unali mbali ya East Germany . Ni njila ina iti imene timaonetsela kuti timayamikila dipo ? Analinso na acibululu ambili mumzindawu . 20 : 18 . Zozizwitsa za Yesu zimaonetsa kuti iye amatikonda ndiponso amakhudzidwa ndi mavuto athu . Muyenelanso kudziŵa zimene zimawacititsa kukaikila . Mphatso ya kuyankhidwa kwa mapemphelo . Palibe cimene Mdyelekezi angacite kuti alepheletse anthu onse olapa moona mtima kudzakhala m’banja la Yehova . Ndipo m’masana , n’nali kugwila nchito zimodzi - modzi . Mnyamata wina wa zaka 15 ku Denmark anati : “ N’tauza makolo anga kuti nikaikila ngati cipembedzo cathu n’coona , anacita nane modekha ngakhale kuti mumtima anali ndi nkhawa . N’cimodzi - modzi ndi makolo amene ali ndi nzelu zopindulitsa . Mmene mungalele bwino ana Pali kugwilizana kwakukulu pakati pa Lemba la Genesis 3 : 15 , mwambo wa Pasika , ndi kubwela kwa Mesiya . Mwacidziŵikile , Danieli anaphunzitsidwa bwino na makolo ake . Mwacitsanzo , Ernesto wa zaka 74 wa ku Philippines , amapita ku laibulale ndi kusankha buku losangalatsa lakuti aŵelenge . Koma ngati khalidwe la anthu ambili layamba kusintha pang’ono - pang’ono , zimakhala zovuta kuzindikila . Nchito imeneyo siinali yopepuka . ( Genesis 12 : 17 ; Numeri 12 : 9 , 10 ; 2 Samueli 24 : 15 ) Yehova analanganso Aisiraeli ndi “ milili ” cifukwa ca kusakhulupilika kwao . Kodi tiphunzilapo ciani pa citsanzo ca Yosefe ? ( Salimo 8 : 3 , 4 ) Ngati nthawi zonse timuuza Mulungu zakukhosi kwathu , timakhala naye paubwenzi wolimba kwambili . — Ŵelengani Yakobo 4 : 8 . Tizipemphela bwanji ? 11 : 16 ; Yobu 31 : 6 . Iye anazindikila kuti njila yabwino koposa imene angakumbukile Mlengi wake Wamkulu ndi kulalikila uthenga wabwino wokamba za Kristu , Mwana wa Mulungu . N’nalekanso khalidwe laciwelewele , kuchova njuga , kumwa moŵa mwaucidakwa , ndi kubela abwana anga . Ndipo kupita kwanu patsogolo ndi kudzipeleka kwanu kudzapindulitsa kwambili Akhiristu anzanu . Yosefe , mtumiki wokhulupilika wa Yehova , anacitilidwa zinthu zopanda cilungamo ndi anthu amene sanali kutumikila Mulungu . Ndipo kulimbana ndi ciyeso cimeneci kunali kovuta . Koma analimbikitsidwa kwambili ndi mlongo Ann , mpainiya mumpingo mwawo . Nthawi zambili Yesu anali kukhala ndi ophunzila ake , ndipo anali kuwaphunzitsa zinthu zokhudza Mulungu . Zikanakhala kuti Francis Woyamba , Mfumu ya ku France sanaloŵelelepo , sembe Lefèvre anapatsidwa mlandu wakuti ni wampatuko . amasamalila zosoŵa zanu ? Kodi iye anacita ciani ? Mosakayikila , nayenso kalembela adzakupemphani fon’namba kapena adresi ya ku mpingo kumene munacokela kuti aitanitse khadi yanu ya Mpingo Yolembapo Nchito za Wofalitsa . Mu July 1942 , pa msinkhu wa zaka 11 , n’nabatizika m’tanki yamadzi pa famu . Pulezidenti Woodrow Wilson wa ku America analimbikitsa mfundo yakuti nkhondo “ idzathandiza kuti ulamulilo wa demokalase ufalikile padziko . ” Kudya zipatso za mtengo umenewo kukanaonetsa kuti io sanali kufuna kuti Yehova aziwalamulila . Ofufuza anapeza kuti akaika gumbwa padzuŵa kapena pamalo a cinyontho , amawonongeka mofulumila . 3 : 15 , 16 ) Pitilizani kuganizila za cikondi ca Mulungu ndi malangizo ake anzelu . Gwen : Maganizo anga onse anali pa nchito yovina . Odzozedwa pamodzi ndi anthu amene ali ndi ciyembekezo ca padziko lapansi ‘ adzaima ’ patsikulo cifukwa cakuti Mulungu adzawavomeleza . Iwo anali kukonza zinthu zonse zofunikila paulendo . Kumeneko , aliyense anagona pa “ makatoni 20 a mabuku oyalidwa bwino monga bedi . ” ( Ŵelengani Chivumbulutso 12 : 7 - 9 , 12 . ) Alongo ena atamva kuti ndifuna kuyamba upainiya , anandiuza kuti ndiyembekeze coyamba kuti makolo anga akhazike mtima pansi . Iye anakamba kuti Davide anamwalila ndipo anaikiwa m’manda . Mwacitsanzo , Mboni ziŵili za ku Australia zinafika pakhomo la mtsikana wina . zofufumitsa ? Nkhani yosamba m’manja ( Maliko 7 : 5 ) , Aug . Onani mmene malangizo anzelu a m’Baibo athandizila anthu kupewa mavuto aakulu zinthu zikalibe kufika poipilatu . Ndiponso mofanana ndi Yehosafati , amene anapita ku dela la Efuraimu kukathandiza anthu kuti ayambenso kulambila Yehova , ifenso tiyenela kuyesetsa kuthandiza anthu amene anazilala . Olivia , wa zaka 17 , amene anabatizika akali wamng’ono , anati : “ Nthawi zambili n’nali kuopa kuti nikaloŵetsa nkhani zokhudza Baibo pa maceza , anzanga adzayamba kuninena kuti ndine wocita zinthu mopambanitsa . ” Tidziŵa bwanji kuti anthu mtsogolo padziko lonse lapansi adzakonda Yehova ndi anzao ? ( Yesaya 33 : 24 ) Ponena za okondedwa athu amene anamwalila amene Mulungu akuwakumbukila , Yesu anakamba kuti : “ Idzafika nthawi pamene onse ali m’manda acikumbutso adzamva mau ake ndipo adzatuluka . ” Iye anati : “ Nonsenu ndinu abale . ” Palibe amene anadziŵa kuti magulu akulu - akulu a asilikali adzamenyana kwa nthawi yaitali ku Belgium ndi ku France . Kuonjezela apo , mmodzi wa alongo anga anakhala Mboni . Conco , Yehova anacititsa cilala m’dzikolo kwa zaka zitatu ndi hafu n’colinga cakuti aonetse kuti Baala ndi wopanda mphamvu . Mfumuyo inapandukila Mulungu ndipo inakhala mfumu yoipa kwambili ya Isiraeli kuposa mafumu ena onse amene analiko iye asanakhale mfumu . Izi zinathandiza kuti nchito yolalikila ipite patsogolo . Yehova anatisamalila kwambili pamene tinaika zinthu za Ufumu patsogolo . Kangapo konse mu umoyo wake , iye analephela kucita zinthu monga munthu wauzimu . ( Mat . Ngati dzila silinatuluke , mimba siingakhale . “ Kuti anthu adziwe kuti inu , amene dzina lanu ndinu Yehova , inu nokha ndinu Wam’mwambamwamba , . . . . pa dziko lonse lapansi . ” — SAL . Cipilala ca Tito ku Rome masiku ano ( Yohane 6 : 22 - 24 ) Iye anadziŵa kuti cifukwa cacikulu cimene io anali kumufunila cinali cakuti awapatse cakudya , osati kuti amve zimene anali kuphunzitsa . Conco , tili ndi cidalilo cakuti adzacotsapo kuvutika ndi cisalungamo . Koma akulu - akulu a chechi anali kuletselatu kumasulila Mau a Mulungu m’zinenelo zimene anthu analukamba . Cifukwa ca ici , akulu - akulu a chechi okha , na anthu ŵena ophunzila ndiwo anali kukwanitsa kuŵelenga Baibo . Makonzedwe amenewa ndi ofanana ndi a m’nthawi ya atumwi . Buku limeneli akuligaŵila mu ulaliki ndipo anthu ambili amene sadziŵa Baibulo akusangalala nalo . — 2 / 15 , tsamba 3 . Kyung - sook anati : “ Nditauzidwa kuti ndili ndimatendawa , ndinakhumudwa kwambili . ( Maliko 13 : 10 ) Iwo akhala mbali ya anthu a Mulungu , ndipo akhala “ gulu limodzi ” ndi odzozedwa , lotsogoleledwa ndi “ m’busa wabwino , ” Kristu Yesu . — Ŵelengani Yohane 10 : 14 - 16 . ( Yesaya 1 : 15 ) Koma anthu a conco ‘ angakhalenso pa ubwenzi wabwino ’ na Mulungu ngati asintha makhalidwe awo . — Yesaya 1 : 18 . Yobu anaika maganizo ake onse pa nkhawa zake , cakuti analephela kuona zinthu monga mmene Yehova anali kuzionela . Ine sin’nalakwe ciliconse . . . . Pewani maganizo amene anthu ambili a m’dzikoli ali nawo , akuti ana afunika kupezela makolo awo zinthu zambili kuti akhale na umoyo wawofu - wofu . Iye ayenela kuti amakondwela kwambili akaona anthu akulambila makolo ao , cilengedwe , nyama kapena zinthu zina osati Yehova , amene ‘ amafuna kuti anthu azidzipeleka kwa iye yekha . ’ ( Eks . Mfundo imene imanithandiza tsiku lililonse ni yakuti : “ Pa zinthu zonse , ndimapeza mphamvu kucokela kwa iye amene amandipatsa mphamvu . ” Ocita kafukufuku anapeza kuti akuluakulu a mumzindawo analandila ciphuphu kuti alole anthu ogwila nchito yomanga kugwilitsila nchito zipangizo zosalimba pomanga sitoloyo ndiponso kuti asatsatile malamulo a kamangidwe kovomelezeka . Ndipo n’zotheka ndithu kupambana pa nkhondo yolimbana ndi zilako - lako zoipazi . Mulungu , amene ndi wanzelu zozama , anapeza njila yabwino kwambili yothetsela nkhanizo , iye sanatisiye cabe kuti tikhumudwe . ( Machitidwe 17 : 3 , 4 ; 20 : 20 ) Ici ndiye cifukwa cimodzi cinacititsa Ayuda “ kusuliza Baibo ya Septuagint , ” malinga na zimene katswili wina wa Baibo dzina lake F . ( b ) Kodi odzozedwa aonetsa bwanji kuti alabadila mau akuti : “ Mkwati uja wafika ” ? Conco ndinauza mkazi wanga ndi ana anga kuti abisale munthoci zimene zinali pafupi . Koma kumbukilani kuti cofunika ngako si kukhala na zinthu zapamwamba pa nyumba . Danieli 12 : 9 . Palinso njila zina zimene tingathandizile mpingo wathu . Pamene Yesu anali padziko lapansi , atsogoleli azipembedzo anali kukonda kupeleka mapemphelo odzionetsela . ( Mat . 7 : 13 ) Yaciŵili , anthu amene amasankha kukhala ku mbali ya Satana sapindula kweni - kweni . Iye anatsegula Baibulo lake la zilembo za akhungu ndi kuyamba kuŵelenga . Kuti mukhale mphunzitsi wabwino , coyamba Mau a Mulungu ayenela kukhala pamtima panu ( Onani ndime 17 ) Buku imeneyi ipezekanso pa www.jw.org . Kuwonjezela apo , m’bukuli anaikamo nyimbo zatsopano zokamba za nchito yathu yolalikila , ndiponso zoyamikila dipo la Yesu . Ndine wokondwela kudziŵana ndi kuyanjana ndi anzake a mkazi wanga cifukwa onse amalambila Yehova . 6 : 6 - 10 . Iye ananyengelela mneneli wa Mulungu wacicepelepoyo ndi kum’pangitsa kutaya malangizo ofunika a Yehova , akuti ‘ asakadye cakudya kapena kumwa madzi , ndi akuti ‘ asakadzele njila imene adutse popita . ’ ( Aroma 7 : 25 ) N’zoonekelatu kuti tingasoceletsedwe ngati tilola mtima kutilamulila pamene tipanga zosankha zofunika kwambili . Koma Maria anakana . Mwacitsanzo , ponena za abale na alongo athu m’nthawi ya ulamulilo wa Nazi ku Germany , munthu wina dzina lake Anton Gill analemba kuti : “ Mboni za Yehova zinali kudedwa kwambili ndi cipani ca Nazi . . . . Mulungu analonjeza kuti adzacotsapo mavuto na kupanda cilungamo . Adzapanga zinthu zonse kukhala zatsopano . — Chivumbulutso 21 : 4 , 5 . Banja la Beteli limathandiza kupeleka cakudya cauzimu . Tiyenela kuonetsa mwa zocita zathu kuti timaona misonkhano kukhala yofunika kwambili . Tikatelo , timapatsa Yehova cifukwa cina cosungila dzina lathu ‘ m’buku la cikumbutso , ’ kapena kuti “ buku la moyo , ” limene mumalembedwa maina a anthu amene akuyembekezela kukalandila moyo wosatha . — Mal . Patapita milungu yocepa , M’bale Joseph F . Yehova nayenso amacita cidwi ndi atumiki ake padziko lapansi . Kuti tikwanitse kucita zimenezi , tifunika kuganizila zitsanzo za anthu akale amene anacita zinthu molimba mtima . Koma izi sizitanthauza kuti kukhala woyamba kubadwa kunalibe phindu . ( b ) N’cifukwa ciani mau a pa Salimo 32 : 8 ndi olimbikitsa kwa aja amene amadzikaikila ? Kuphika mkate . Tizitsatila Khalidwe Lopambana . Malinga ndi lemba la Genesis , Yehova anachula zinthu zitatu ziti ponena za anthu ? Mau a Mulungu amapeleka uphungu wanzelu kwa onse oloŵa m’banja . Ndipo m’pake , cifukwa amene anayambitsa cikwati amafuna kuti onse okwatilana akhale acimwemwe . ( Miy . Ngati munthu amene amadziŵa zanyengo wakhala wodalilika kwa nthawi yaitali mungam’dalile . Iye anachula zinthu monga zilakolako zoipa ndi kukondela ndi zina zotelo . ( Mateyu 6 : 9 ) Conco , Yehova ndi Atate wathu ndipo amatikonda monga mmene tate wabwino amakondela ana ake . Tikasonkhana , timaonetsa kuti timafuna kuceza ndi abale athu ndiponso kudziŵa mmene zinthu zilili paumoyo wao . Mungandionetse . ( Salimo 53 : 2 ) Mwacitsanzo , tsiku lina pamene Allan anali kulalikila pacilumba ca ku Philippines , anakumana ndi mai wina . Ngati tilemekeza olamulila aboma , iwo angatilole kupitiliza kugwila nchito yolalikila mwaufulu . Koma ca m’ma 1800 , asayansi anakhazikitsa ciphunzitso cina . 15 : 1 - 21 ) Cimodzi mwa zinthu zabwino zimene tikuyembekezela ndi ciyembekezo cathu cotsimikizilika cakuti tidzapulumutsidwa ku mavuto onse amene timakumana nao . ( Sal . 37 : 9 - 11 ; Yes . Parkin ( Ŵelengani Genesis 22 : 15 - 18 ; Aheberi 11 : 17 . ) ANTHU ENA AMAKAMBA KUTI alibe dzina , ena amati dzina lake ndi Mulungu kapena Ambuye , ndipo ena amati ali ndi maina ambili . Hana analonjeza kuti akadzabeleka mwana , mwanayo adzakhala Mnazili kwa moyo wake wonse , kutanthauza kuti adzapatulidwa ndi kupelekedwa kwa Yehova kuti nchito yake ikhale kutumikila iye basi . — Num . Komanso pofika mu m’badwo wacitatu , anthu anayamba kucita zinthu zoipa ngako . ZAKA zambili zapitazo , mng’ono wanga , Araceli anakwiya kwambili ndipo anandinyoza . Conco mwathandizo la Yehova ndi citetetezo cake , “ Yoswa anagonjetsa Aamaleki ndi anthu amene anali kumbali yao . ” ( Eks . 5 : 11 ) Inde , Yehova adzakondwela kwambili ngati tonse ‘ tipitiliza kulimbikitsana tsiku na tsiku . ’ Anzake ambili anali atapita ku maiko ena kukafunafuna ndalama zambili . N’ZOKONDWELETSA cotani nanga kuona mmene gulu la Yehova likupitila patsogolo ! Ngakhale pamene abale 8 amenewo anali m’ndende , sanagwedezeke pa cikhulupililo cawo ca m’Malemba . 12 : 9 ) Poseŵenzetsa cipembedzo conama , iye amafalitsa mabodza ponena za Yehova . Monga tidziŵila , Danieli anapitiliza kukamba na Mulungu m’pemphelo nthawi zonse . Mwacitsanzo , mu 2008 , kunayamba Sukulu ya Akulu . Pamene tinadziŵa Yehova , ise mofanana ndi Paulo , tinasiya zinthu zina zimene zikanaticititsa kukhala wodziŵika kwambili m’dziko la Satanali . Iye anati : “ Ndikayamba kuganiza molakwika ponena za nchito imene ndinapatsidwa , ndimangoziuza kuti : ‘ Iwe fumbi lacabecabe , uli ndi ciani conyadila ? ’ ” Iye anati : “ Poyamba sin’nali womasuka na abale na alongo . Ponena za Yehova , wamasalimo anati : “ Mumatambasula dzanja lanu ndi kukhutilitsa zokhumba za camoyo ciliconse . ” 6 : 33 ) , 9 / 15 Akacita zimenezi , mkazi wake amamva kukhala wotetezeka , amacita kumva bwino kulemekeza mwamuna wake , kum’cilikiza , ndi kum’gonjela . Masiku ano , anthu ambili ali na makhalidwe ngati amene Akhristu atatu amenewa anali nawo poyamba . “ Pamenepo , anthuwo anayamba kulimba mtima cifukwa ca mau [ ake ] . ” — Ŵelengani 2 Mbiri 32 : 6 - 8 . Makonzedwe amenewa akutiuza zambili za Yehova . 13 : 4 ) Nanga bwanji za kupatukana ndi mnzako wa m’cikwati , osati kusudzulana ? Koma kukamba zoona , “ cikhulupililo sicikhala ndi anthu onse . ” Mwacibadwa , timafuna kudziŵa ngati cimene tifuna kucita cili ndi phindu lililonse . ( Aroma 9 : 21 ; 1 Akorinto 6 : 9 - 11 ) Pamene anali kuphunzila Malemba , analimbitsa cikhulupililo cawo mwa Yehova ndipo anamulola kuti awaumbe . Koma nditapita kukoleji , ndinasiya kupemphela . Yesu sanali kugwilizana ndi khalidwe loona mtundu wa Ayuda kukhala wapamwamba kuposa mitundu ina . 20 : 1 - 3 , 6 . Komanso , anchito odzifunila zungulile dziko lonse ali kaliki - liki pa nchito yomanga Nyumba za Ufumu ndi kuwonjezela maofesi a nthambi . Zonsezi zikucitika pansi pa uyang’anilo wa dipatimenti ya zomanga - manga ( Worldwide Design / Construction Department ) . Tiyeni tikhale otsimikiza mtima kugwilitsila nchito mphatso iliyonse imene Yehova watipatsa , kuphatikizapo Baibulo limene limalemekeza dzina lake . Tera atate wawo , anapita ndi Abulahamu na Sara , olo kuti anali na zaka pafupi - fupi 200 . Mwina si mtumiki wothandiza , koma adziŵa kuti afunika kukhala na makhalidwe amene mzimu woyela umatulutsa . Masiku ano , akatswili amafufuza zocitika za padziko lonse , na kufotokoza zimene zidzacitika m’tsogolo . Espen ndi Janne amakhala m’dziko lolemela la ku Ulaya . Cilamulo cinakambanso kuti munthu akalonjeza kwa Yehova , “ asalephele kukwanilitsa mau ake . Abale na alongo akaona kuti ndinu wodzipeleka , adzayamba kugwilizana namwe . ” Limaika oyang’anila dela ndi abale a m’Komiti ya Nthambi . ( 1 Petulo 5 : 6 ) Conco , ngati zimene timapempha siziyankhidwa mwamsanga , tisaone monga kuti Yehova sasamala za ife . N’nayamba kugwila nchito ya zamagetsi m’migodi . Ganizilani mfundo izi : Ife sitili pansi pa Cilamulo ca Mose . Nikaganizila umoyo wanga kucokela pamene n’nali kuyembekezela kubatizika m’cibafa comwelamo ziweto cija , nimayamikila Yehova cifukwa ca anthu anzelu amene ananithandiza poyenda m’njila ya coonadi . Kodi kulankhulana bwino kungalimbitse bwanji cikwati ? 10 : 22 . Ngati tidalila Yehova , tidzakhala olimba . Iye sanalole kuti zimenezi zim’sokoneze kuphunzitsa ophunzila ake . Kumwetulila kudzacititsa ena kuyamba kumasuka nanu . Palipano , pali abale na alongo pafupi - fupi 67,000 amene ali m’Gulu la Padziko Lonse la Atumiki Apadela a Mboni za Yehova . N’zitsanzo ziti za m’nthawi ya atumwi zimene zionetsa kuti anthu angathe kugonjetsa tsankho ? Cifukwa cakuti Sebina anayamba kudzifunila ulemelelo , Mulungu ‘ anamucotsa pa udindo wake ” na kuikapo Eliyakimu . ( Yes . Iwo akaukitsidwa , amakumbukilabe umoyo wao wakale akali padziko lapansi . NYIMBO : 41 , 69 ( Genesis 24 : 59 - 61 ; 35 : 8 ) Atayenda mtunda ndithu , dziko la Harana linayamba kubisika . Ni madalitso ati amene adzatheka mu ulamulilo wa Ufumu wa Mulungu cifukwa ca dipo ? 13 : 2 ) Kumbukilaninso kuti mtumwi Paulo anali kudela ‘ nkhawa mipingo yonse . ’ ( 2 Akor . Mwina na imwe mwafika povomeleza kuti moyo ni waufupi , wodzala na mavuto . Cinthu cofunika kwambili cimene cingatithandize kukhalabe acangu mu utumiki ndi kukhala ndi ndandanda yokhazikika yophunzila Baibulo . Nowa atayenda na Mulungu kwa zaka zoposa 500 , Yehova anam’lamula kuti amange cingalawa copulumutsilamo anthu na nyama . ( Gen . Aisiraeli omwe anali mbadwa za Abulahamu , poyamba anali paubwenzi ndi Yehova ndipo iye anali Atate wao . Kuti anthu aziŵelenga Baibo m’citundu cawo . 3 : 16 ) Zoonadi , “ Yehova amadziŵa anthu ake . ” Koma kumathandiza kwambili kuthetsa mavuto , na kukulitsa cikondi m’banja . Popeza kudzicepetsa kuli ndi maubwino ambili , tingacite bwanji kuti khalidwe limeneli lipitilize kukula mwa ife ? ( Nyimbo 1 : 9 - 11 ; 6 : 10 ) Koma mtsikanayo anakhalabe wokhulupilika kwa m’busa wake wokondedwa . N’cifukwa ciani Mboni zimene zatumikila kwa zaka zambili zimakhulupilila kuti zinapeza coonadi ? Paulo sanadzitame pa zimene anacita asanakhale Mkhristu , ndipo sanakambeko ciliconse cokhudza maonekedwe ake . ( Mac . Ngakhale n’telo , ndinaganiza zakuti ndipemphele kwa Mulungu wa m’Baibulo . Mtumwi Paulo analimbikitsa Akristu anzake ‘ kugwila nchito molimbikila . . . kuti akhale ndi kanthu kena kopatsa munthu wosowa . ’ Ngati n’conco , dziŵani kuti Mulungu amayamikila kwambili zimene munacita . Tikakhala mu ulaliki timakambitsilana ndi anthu osiyanasiyana . Kodi adziŵa kuti mapindu amakhala oculuka kwambili kuposa mavuto ? 2 : 32 ; Mat . Mkazi wanga anandipulumutsa , ndipo anapulumutsanso mwana wathu wamkazi wa zaka 5 kumoto umene unali kuyaka kwambili . Anacilitsa odwala , olemala , osaona , ogontha ndi osalankhula . Posapita nthawi , n’nazindikila kuti a Mboni za Yehova ndiwo okha amalemekeza dzina leni - leni la Mulungu lakuti Yehova na kuliseŵenzetsa . Nanga n’cifukwa ciani afunika kutelo ? Ndi malangizo ati a m’Baibulo amene angathandize Akristu amene akhala kutali ndi mabanja ao ? ( Gen . 8 : 20 ) Mofanana ndi Abele , mosakaikila iye anali kukhulupilila kuti anthu adzamasulidwa ku ukapolo wa ucimo ndi imfa . Kodi iye anaganiza kuti Sara , amene anacoka mumzinda wolemela wa Uri ndi kukakhala m’mahema , angakopeke ndi nyumba zokongola za Farao ndi Abimeleki ? Blessing anati : “ Nthawi zambili n’nali kuganiza zothaŵa , koma n’nali kuopa zimene adzacitila banja lathu . Anapitiliza kuti : “ Coonadi candithandiza kukhala ndi mtima wathunthu kuti Yehova aonetse mphamvu zake kwa ine . Muzikonda nchito iliyonse imene mwapatsidwa mumpingo , kuphatikizapo kupsela . Makhalidwe amaphatikizapo mfundo zimene munthu amasankha kuyendela mu umoyo . ( b ) Kodi tiyenela kukhala otsimikiza mtima kucita ciani ? ( Gen . 1 : 27 ) Conco , munthu aliyense , pamlingo winawake amaonetsa makhalidwe a Mulungu . 34 : 18 ) Panthawi ina , mneneli wokhulupilika Yeremiya anafooka ndi kucita mantha . Koma Jimmy anaona monga kuti amai ake analeka kum’konda . Brian anati : “ Kuona anthu ambili akumvetsela uthenga wa Ufumu ndi kuona cikondi cimene abale ndi alongo akuonetsa , zimalimbikitsa kuti ukatumikile kudziko lina . ” Tinali kufunika kucoka pamalo ena ake pambuyo pa milungu ingapo . Conco , tinali kupempha anthu acidwi kwambili kuti apitilize kuphunzitsa ena mpaka pamene tidzabwelelanso . Arthur na anzakewo anakhala m’malo awo n’kumayembekezela cizindikilo cowadziŵitsa kuti adule nthambozo . Pali malangizo ambili amene angathandize munthu kupilila cisoni . Kudzipeleka kwa Yesu kuti afe ali wokhulupilika kwaYehova , kumakhudza nkhani zofunika kwambili kwa zolengedwa za kumwamba ndi padziko lapansi . — Aheb . Conco , mulekeni asaine apa kuti ndi wa Mboni za Yehova , ndipo timutumiza ku Lilongwe kuti akamumange . ” Koma izi sizinalepheletse abale kuticitila zabwino . Kutumikila Yehova ndi mwai wamtengo wapatali ndipo timasangala kumutumikila . Ubwenzi umenewu umatheka cifukwa cakuti Mulungu amatikonda ndipo ngati ife tili ndi cikhulupililo mwa iye ndi mwana wake . Pa cifukwa cimeneci , anaonedwa monga adani a Boma la Germany , ndipo anazunzidwa kwambili . Komabe , Baibulo limaonetsa kuti mpingo uyenela kucita zonse zimene ungathe kuthandiza Akristu okalamba . Kudzipeleka kwa Mulungu kwa Jairo kunadziŵika ndi aphunzitsi a pasukulu pake . M’dziko lamtendele limenelo , anthu omvela adzamasuka pang’onopang’ono ku ucimo . — Aroma 6 : 17 , 18 ; 8 : 21 . ( Yohane 11 : 11 - 14 ) Conco , palibe cifukwa coopela anthu amene ali m’tulo twa imfa , kapena kuwakondweletsa mwa kuwapelekela mphatso . Madison , wa zaka 15 , anati “ Cimanivuta kutsatila miyezo ya Yehova kuti n’satengele zimene anzanga amaona kuti ndiye zabwino kapena zokondweletsa . ” Nanga lingakupindulitseni bwanji ? Ngakhale kuti Mulungu anamucitila zinthu zabwino , Solomo ananyalanyaza lamulo la Mulungu lakuti asakwatile akazi a mitundu yowazungulila amene sanali kulambila Yehova . KUKHUMUDWA NGATI SUNACIPEZE CIMWEMWE CIMENE UNALI KUYEMBEKEZELA . Aug . 11 : 9 ; 25 : 8 ; 33 : 24 ; 35 : 5 - 7 ; 65 : 22 . Mwacitsanzo , ena asankha kupatukana poona kuti moyo wawo wauzimu kapena wakuthupi uli pa ciopsezo cacikulu cifukwa mnzawo wa m’cikwati ndi wankhanza kapena wampatuko . M’baleyo sanangopatsa munthuyo magazini atsopano a Nsanja ya Mlonda n’kucoka , koma anamuŵelengela lemba limodzi la m’magaziniyo . INE ndi Gwen tinayamba kuphunzila kuvina tili ndi zaka zisanu . Mukakhumudwitsa munthu wina , muzivomeleza na kupepesa mwamsanga . 7 : 21 , 22 ) Mofanana ndi inu , ionso anali kukhala m’nthawi yapadela . Ulendo wanga woyamba woyendela nthambi , ku Venezuela , mu 1970 ( Ŵelengani Genesis 1 : 28 . ) Zotulukapo zake zinali zakuti ciŵelengelo ca apainiya a nthawi zonse ku Turkey cinawonjezeka . Yehova watipatsa Mau ake , Baibo . Margaret , ca m’ma 1968 Iye anati : “ Tsopano ndili ndi moyo waphindu , osati cifukwa copita kunyumba ndi nyumba kupemphetsa ndalama za cipani , koma cifukwa colalikila za Ufumu wa Mulungu , umene udzabweletsa cilungamo padziko lapansi . ” Satana amakamba kuti Yehova si woyenela kutilamulila . Nthawi yomweyo khate lakelo linatha . ” Ponena za anthuwo , Yesu anati : “ Mocenjela , mumakankhila pambali malamulo a Mulungu kuti musunge mwambo wanu . ” Yesu anali ndi “ angelo ake ” nthawi yoyamba imene anamangilila lupanga lake m’ciuno kuti athamangitse Satana ndi ziwanda zake kumwamba . ( Chiv . Ndipo panthawiyo , “ palibe munthu wokhala m’dzikolo amene adzanene kuti ndikudwala . ” — Yesaya 33 : 24 . 6 : 2 - 4 , 11 , 12 ) Koma Nowa anali munthu wolungama . Mwacitsanzo , abwana anu kunchito angamakupempheni kaŵili - kaŵili kuti mugwile nchito ya ovataimu m’madzulo kapena kumapeto kwa wiki , nthawi imene mumacita kulambila kwa pabanja , kupita mu ulaliki , ndi kupezeka pa misonkhano . Kodi ndi anthu otani amene tifunika kucita nao zimenezo ? Masiku ano tili ndi umboni wamphamvu woonetsa cifukwa cake tiyenela kugwilitsila nchito dzina la Yehova . N’ciani cimene wophunzila Yakobo anafotokoza pokamba za cikhulupililo ca Mkhiristu woona ? Koma ca m’ma 1800 , mabungwe ena anamasulila Baibulo kapena kulisindikiza m’zinenelo pafupifupi 400 . Acinyamata — Kodi Mungakonzekele Bwanji Ubatizo ? Maganizo a dziko amapangitsa munthu kunyalanyaza kapena kupeputsa malangizo a Yehova . Kumbukilani kuti tikucita cifunilo ca Mulungu , ndipo tikuyembekezela mwacidwi moyo wosatha . Komabe , nthawi zonse n’nali kukhala mwamantha , cifukwa n’nadziŵa kuti sinidzapewa zotulukapo za chimo langa . KONZEKELANI “ MASIKU OIPA ” Kodi mabanja angacite ciani pamene makolo okalamba afunikila thandizo ? ( b ) Ndi citsanzo cotani cimene Yesu anatisiila ? Kodi io akanacita ciani ? ( Aheb . 5 : 14 ) Iwo amaonetsa kuti akukula kuuzimu mwa kupanga zosankha mwanzelu , olo pamene makolo awo kapena anthu ena aakulu sakuwaona . ( Afil . 21 : 12 , 13 ; Yoh . 2 : 14 - 17 . Iwo angakhale kuti sanacite chimo lalikulu moti n’kupatsidwa cilango mu mpingo . Zofanana ndi zimenezi zinacitikanso m’nthawi ya mtumwi Paulo patapita zaka 1500 . Pikica ya m’magazini ya mu 1944 yochedwa La Nación , yoonetsa abale akuyenda atavala zikwangwani ku Mexico City Mosakaikila , mumafuna kulemekezedwa . Tapanga ubwenzi wathithithi ndi io , ndipo timadalilana ndi kulemekezana . ” Nkhani yaciŵili idzaonetsa mmene tingatengele citsanzo cake pankhani yokhala wolimba mtima ndi wozindikila . Mwanayo aganizila zimene atate ake amuuza kenako afunsa kuti : “ Atate , kodi ndani anapanga Mulungu ? ” 13 : 5 - 9 . Nthawi zambili zimene munthuyo angakambe zingacititse kuti akambilane zambili za m’Baibulo . ( Luka 12 : 48 ) Komabe , ngati timakonda Yehova na mtima wonse , palibe cimene cidzatipunthwitsa kapena kutilekanitsa na cikondi cake . — Sal . Sascha Pakuti si nzelu kufunsa funso lotele . ” — Mlal . Kodi tingakupewe ? Koma pambuyo pake , Yona anamvela ndi kupita ku Nineve . ( Aroma 12 : 2 ) Pang’ono ndi pang’ono , ndinayamba kusintha . Acicepele amakula , koma osadziŵa maluso ofunikila kuti akhale na umoyo wabwino . Kodi adani athu tiyenela kuwaona bwanji ? Hana anakhutulila Yehova za mumtima mwake . Imakamba kuti iye sanagwilizane ndi ciwembu cimene Khoti Lalikulu la Ayuda linakonzela Yesu . ( Yohane 14 : 9 ) Ena amakonda mabuku a maulosi monga la Chivumbulutso , limene limakamba “ zinthu zimene ziyenela kucitika posacedwapa . ” Olo kuti anali atatumikila Mulungu mokhulupilika zaka zambili , Yehova anauza Mose kuti amulimbikitse . Kodi acinyamata angapindule bwanji cifukwa cokhala paubwenzi ndi Akristu ofikapo ? Coyamba , anthu odziletsa sakhala na mavuto ambili . N’zodziŵikilatu kuti simungaloŵe m’gulu la anthu amenewo . Koma kodi mungayambe kuganiza kuti anthuwo acita bwino ? Mukamakonzekela phunzilo la Baibulo mwa njila imeneyo , cikhulupililo canu cidzalimba . Mudzayamba kuphunzitsa mogwila mtima . Zimene Satana Mdyelekezi anacita zinayambitsa cikayikilo cakuti kaya Yehova ni woyeneladi kulamulila kapena ayi . Palibe lamulo lacindunji la m’Malemba lotiletsa kukapezekapo . Koma m’Baibulo muli mfundo zina zimene zingatithandize kupanga cosankha . 3 Anadzipeleka na Mtima Wonse — Ku Turkey Conco , iye sananyengedwe ndi ‘ zosangalatsa zosakhalitsa zaucimo . ’ Kuti mudziŵe zambili , onani “ Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi ” mu Nsanja ya Mlonda ya May 15 , 2015 , mape . Monga mmene takambilana kale , kupitila m’dipo Yehova amatenga Akhiristu odzozedwa kukhala ana ake . ( Mat . 5 : 11 , 12 ) Ululu utafika ponyanya , n’nakomoka . Kusunga cakukhosi kungalepheletse m’bale kutumikilanso monga mkulu . Nyumba ya Ufumu ndi nyumba yopelekedwa kwa Yehova . Kale , tinali kukonda kukamba kuti nkhani zina zinali kuimila zinthu zazikulu zimene zinali kudzacitika mtsogolo . Conco , dzifunseni kuti : ‘ Nikamaŵelenga Baibulo , kodi nimasinkhasinkha ndi kulola malangizo a Mulungu kusintha maganizo ndi mtima wanga ? Posacedwa , iwo adzawononga mitundu ya anthu ndi kuthetsa kuipa konse . — Ezekieli 10 : 2 , 6 , 7 ; Chivumbulutso 19 : 11 - 21 . N’naona kuti zinthu zambili zimene Mulungu analosela , zinacitikadi ngakhale kuti anakamba kukali zaka zambili . ( Yoh . 6 : 40 , 44 ) M’paradaiso , Yesu adzakwanilitsa udindo wake monga “ kuuka ndi moyo . ” — Yoh . 4 : 19 , 20 ) Ngakhale n’conco , m’kupita kwa nthawi anawo adzafunika kupanga okha cosankha pankhani ya kulambila . — Deut . Palibe mphatso ina imene anatailapo zambili kuposa iyi . Mwacitsanzo , nthawi ina pamene ndinali kulalikila kunyumba ndi nyumba , ndinapitikitsa mbala imene inaba wailesi ya m’galimoto yanga . Conco , n’naleka kumvetsela nyimbo zimenezo . Pofuna kupewa kukhala woledzela , n’naleka kupita ku mapati na ku manaitikilabu , cifukwa nikapita kumeneko n’nali kukakamizika kumwa mowa kwambili . Ngakhale kuti Baibo pokamba za angelo imawachula monga amuna , ndipo poonekela kwa anthu akhala akuonekela monga aamuna , kweni - kweni kulibe angelo aamuna kapena aakazi . Ndipo tikayandikila Yehova nayenso adzatiyandikila , tsopano ndi kwamuyaya ! 2 : 24 ) Yehova anakamba mau amenewa pomanga cikwati coyambilila . Yesu anacenjeza kuti aneneli onyenga ‘ adzabwela atavala ngati nkhosa ’ YEHOVA 27 Muziona Kusiyana Pakati pa Anthu Anthu ocokela ku maiko ena afunika kucita zimene angathe kuti agwilizane na cikhalidwe ca m’dziko lacilendo . N’cimodzimodzi ndi cikhulupililo cathu . Mwacionekele , ‘ munthu woipa ’ amene Paulo anachula anali kucita ciwelewele , ndipo analibe mantha kapena manyazi . Mwacitsanzo , anali kulalikila m’miseu ndi m’misika . Yaciŵili , “ Mulungu ndi wokhulupilika . ” Iye anati : “ Nonse mupeleke zopeleka kwa Yehova . Iye anasimba kuti : “ Kutumikila ku dziko lina kwanipatsa mwayi wodzionela nekha mmene Yehova akukopela anthu a mafuko ndi zikhalidwe zonse kubwela m’gulu lake . Mulungu anakupatsani dipo la nsembe ? Kuyambila kale , anthu akhala akulakalaka kukhala acinyamata kosatha ndiponso kukhala ndi umoyo wathanzi labwino . ( Agal . 4 : 22 - 25 ) Komabe , pa kukwanilitsidwa kwakukulu kwa ulosi umenewu , monga mmene mtumwi Paulo anafotokozela mouzilidwa , mbali yoyamba ya mbeu ya Abulahamu ndi Kristu . Ndipo mbali yaciŵili ndi Akristu a 144,000 odzozedwa ndi mzimu . ( Agal . 3 : 16 , 29 ; Chiv . Mbali yoyamba ya lembali limati : “ Koma kwa ine kuyandikila kwa Mulungu ndi cinthu cabwino . ” Kodi n’ciani cinapangitsa Eliya kukhala ndi maganizo amenewo ? 14 KODI N’KUPHONYA CABE PA KAMVEDWE ? Cilamuloco cinapeleka malangizo a zimene munthu angacite kuti akhalenso woyela . Komabe , kuyambila pa zinthu zomwezo zimene zinam’pweteka mtima , Paulo anacitila umboni mogwila mtima . 1 : 12 - 14 . N’zosakayikitsa kuti zimene Boazi anacitila Rute mkazi wacimoabu zinaonetsa mmene Yehova amaonela alendo . Komanso iwo amauluka paliŵilo lalikulu kupambana liŵilo la cinthu ciliconse ca padziko lapansi kapena ca kuthambo . — Salimo 103 : 20 ; Danieli 9 : 20 - 23 . Cifukwa cimodzi cimene asilikali aciroma anali kucitila bwino pa nkhondo , n’cakuti tsiku lililonse anali kuyeseza mmene angaseŵenzetsele malupanga awo . Ndipo muziyelekezela kuti muli m’dziko latsopano . Baibulo limati iye “ anakana kuchedwa mwana wa mwana wamkazi wa Farao , ndipo anasankha kuzunzidwa pamodzi ndi anthu a Mulungu , m’malo mocita zinthu zosangalatsa koma zosakhalitsa zaucimo . ” Kodi ofalitsa amacita bwanji na vuto limeneli la kucepa kwa gawo ? Zikatelo , mungapite kwa dokotala kuti akakupimeni , popeza kuti nkhawa nthawi zina zimakhala ciyambi ca matenda ena ake . Iye anakhalabe wokhulupilika ku Cilamulo ca Yehova mosasamala kanthu kuti olamulila ankhanza anamuzunza kwambili . ( Num . 36 : 7 ; 1 Maf . Nyimbo zimenezi zimakonzewa m’njila yakuti zitithandize kukonzekeletsa mitima na maganizo athu kaamba ka pulogilamu ya msonkhano . Ndipo ena amaona kuti m’pofunika kuiyeletsa kokha ngati kumaloko kulibe miseu yabwino ndiponso kumacita matika kapena fumbi . Komanso ena amanyalanyaza nchitoyi cifukwa cakuti kumaloko kulibe madzi okwanila kapena zipangizo zogwilitsila nchito . Kodi uphungu umene Yehova amapeleka kupyolela mwa atumiki ake , umaonetsa bwanji kuti amatisamalila kwambili ? O’Connor anabwelanso ku Dublin ndi mnzake wacipembedzo , amene anayambanso kufunsa mafunso otsutsa . Ngati Yehova amaona zolengedwa zake zopanda moyo kukhala zofunika , kuli bwanji ise anthu , amene timam’tumikila modzifunila cifukwa com’konda ? ( Sal . Kwa zaka zambili , zofalitsa zathu zakhala zikufotokoza kuti munthu , kapena mbuye wa m’fanizoli ndi Yesu , ndi kuti anapita ku dziko lakutali pamene anakwela kumwamba mu 33 C.E . Kodi Mfumu yoipa Ahabu analephela kukhulupilila ciani ? 2 : 10 , 11 . Koma ngakhale kuti zinthu zinali conco , tonse tinali kupezeka pa misonkano yonse ya mpingo ndi kupita mu utumiki mokhazikika . ” Kuseŵenzetsa cuma pocilikiza zinthu za Ufumu kumaonetsa kuti ndise ‘ anzelu ’ m’njila inanso . Mu 1950 , ine ndiye n’nali wamng’ono kwambili pa ofesi yathu ya nthambi . Iwo ananditumizila munthu woyenelela kudzandiphunzitsa Baibulo . Conco , ambili amakonda kucita zinthu zimene amaona kuti n’zoyenela kwa iwo , ndipo safuna kutsatila miyezo ya Mulungu . Anthu ena amaona ngati mkaziyu anacita zinthu modzikuza , koma Yesu anaona kuti mkaziyo anali wovutika . Pambuyo poona masomphenya a ulemelelo wa Mulungu , mneneliyu anakamba za kupanda ungwilo kwake kuti : “ Tsoka kwa ine ! Pamene anali kumufunsa , wansembeyo anakwiya ngako cakuti anam’ponyela Baibo , uku akukalipa , amvekele : “ Wasanduka Satana iwe ! Iye anati : “ Zinali zovuta kwambili . 3 : 9 ) Conco , tifunika kumakamba zoona ngakhale kuti kucita zimenezo nthawi zina kungakhale kocititsa manyazi . — Miy . 17 : 45 , 49 , 50 . Pilato anawayankha kuti : “ Inu muli nao asilikali olondela . Koma mosiyanako , mamembala a Khoti Yapamwamba ya Ayuda anaimba mlandu Sitefano , ndi kumupha mwa kum’ponya miyala . — Mac . Akulu masiku ano afunika kuyesetsa kutengela Yehova , Mulungu amene “ amakonda cilungamo . ” Ganizilani citsanzo ca wacicepele wina wa ku France dzina lake Rico . Atate wake amene si Mboni , sanafune kuti iye abatizike , ndipo zimenezi zinam’fooketsa . Cinanso , pamafunika ndalama zoculukilapo zosamalila mayi woyembekezela na mwana amene adzabadwa . 94 : 19 . Muyenela kukonzekela tsogolo lanu ndi kukhulupilila malonjezo a Mulungu . 24 : 36 ) Koma apa Yesu kumwamba anapatsidwa mphamvu zowononga dziko la Satana . Yesu anati : “ Ngati mumandikonda , mudzasunga malamulo anga . ” Mau amenewa amasonyeza kuti ulosi umenewu udzakwanilitsidwadi . Ndi udindo wotani umene Mulungu anapatsa Mariya ? Ndiye cifukwa cake , tiyenela ‘ kuvula colemela ciliconse ndi . . . kuthamanga mopilila mpikisano umene atiikila . ’ Kodi cuma cakuthupi tingaciseŵenzetse bwanji kuti tilimbitse ubwenzi wathu na Mulungu ? Onani zinthu 6 zimene zimatsimikizila kuti Ufumu wa Mulungu udzathetsa ziphuphu . Conco , m’kupita kwa nthawi ndinayamba kukhala ndi umoyo wosalila zambili . Iye anati : “ Ukatelo Atate wako amene amaona kucokela kosaonekako adzakubwezela . ” Iye anati : “ N’nayamba kukonda kwambili anthu amene n’nali kuphunzila nawo Baibo , ndipo n’nali kumva bwino kuwaona akukhala atumiki okhulupilika a Yehova . M’BAIBULO , muli malamulo omveka bwino amene Yehova watipatsa okamba zimene tiyenela kucita ndi zimene tiyenela kupewa . Paulo anauza abale a ku mpingo wa ku Roma kuti : “ Ngati ukulengeza kwa anthu ‘ mau amene ali m’kamwa mwakowo , ’ akuti Yesu ndiye Ambuye , ndipo mumtima mwako ukukhulupilila kuti Mulungu anamuukitsa kwa akufa , udzapulumuka . ( Gen . 13 : 15 - 17 ; 17 : 1 - 8 , 16 ) Abulahamu anali ndi cikhulupililo cosagwedela m’malonjezo a Mulungu cakuti anali wofunitsitsa kupeleka nsembe mwana wake wobadwa yekha . Yesu anali kukondanso Mariya amai ake . Ndipo ambili amafuna kumva mau monga a kuciyambi kwa nkhani ino kucokela kwa wolandila mphatsoyo . N’zacisoni kuti okwatilana ena amalephela kusonyezana cikondi , ndipo amuna ena amaganiza kuti koonetsa cikondi mkazi n’kumupusika . Colinga cathu cinali cakuti tidzapite ku Sydney , m’dziko la Australia , kumene amalume anali kukhala . Makolo pamodzi ndi mwana wawo angaŵelenge buku lakuti Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa — Buku Lachiwiri , peji 304 mpaka 310 . ( 1 Akor . 7 : 5 ) Zingakhale zomvetsa cisoni ngati okwatilana angalole Satana kugwilitsila nchito ‘ kulephela kudzigwila ’ kwao kuti acite cigololo . Muzifuna - funa ‘ cuma cakumwamba , ’ kapena kuti ciyanjo ca Yehova , osati “ ulemelelo wa anthu . ” — Ŵelengani Maliko 10 : 21 , 22 ; Yoh . 12 : 43 . Kukamba mokoma mtima : Timakamba ndi anthu mokoma mtima cifukwa cakuti timawalemekeza . Ganizilani zosoŵa za wophunzila wanu , ndipo pezani funso kapena fanizo limene lidzamuthandiza kupita patsogolo . Ngati timaona utumiki monga cuma camtengo wapatali cocokela kwa Yehova , sitidzakhutila na kupanga cabe maola tikapita mu ulaliki . Mwacitsanzo , poŵelenga nkhani ya Yosefe , yelekezelani m’maganizo mwanu kuti mukuwaona abale ake akumugulitsa kwa Aisimaeli . ( Gen . Nthawi zina anali kulephela kuŵelenga cifukwa ca matendawo , conco anayamba kumvetsela mau ojambulidwa a m’Baibo ndi a m’mabuku ophunzilila Baibo . Anthu ena amakamba kuti cisoni cimasila cokha m’kupita kwa nthawi . Nkhaniyi idzatilimbikitsanso kutsatila zitsanzo za anthu akale amene anasankha kulambila Yehova , Mfumu yamuyaya . ( b ) Kodi kumangiwa kwawo kunawatayitsa cikhulupililo mwa Yehova ? Cikhulupililo cinathandizanso Mose kusankha zocita paumoyo . 8 : 20 ; 9 : 18 , 19 . Tinali kuphunzila Baibulo ndi banja lina la anthu 5 . Kodi ndi kuti kumene banja lingapeze thandizo ? Nyumba yamitengo imene n’nabadwilamo Kodi Mulungu amasamala za ine ? Kuti tikhale pa unansi wabwino ndi ena , ngakhale adani athu , Baibo imatilimbikitsa kukhala oceleza . Baibulo limatiuza kuti : “ Khulupilila Yehova ndi mtima wako wonse , ndipo usadalile luso lako lomvetsa zinthu . Sukuluyi inathandiza ofalitsa onse kukhala alaliki ogwila mtima . M’malomwake , iye anali kukhulupilila kuti Yehova ndi amene adzamuteteza pamodzi ndi banja lake . Satana sakanamva cisoni ngati Sara akanaononga banja lake , mbili yake , ndiponso ubwenzi wake ndi Yehova . Patapita zaka zambili , mtumwi Paulo analemba izi ponena za iye : “ Mwa cikhulupililo , iye anacita pasika ndiponso anawaza magazi pamafelemu a pakhomo , kuti woonongayo asakhudze ana ao oyamba kubadwa . ” ( Aheb . Kukhulupilila Yehova kunathandizanso mlongo wochedwa Ella kupewa msampha woopa anthu . A “ khamu lalikulu ” amenewa amakonda Yehova ndi Mwana wake , ndipo amalambila Yehova “ usana ndi usiku . ” — Chivumbulutso 7 : 9 , 14 , 15 . Izi zimawathandiza kudziŵa mau enieni apaciyambi a m’Baibo . Ubatizo ndi cosankha cacikulu komanso mwai wapadela Koma ngati tiyamba taganiza tisanakambe ciliconse , tidzasankha bwino mau , kuyankha mofatsa , ndipo padzakhala zotulukapo zabwino . Nikukamba nkhani pa msonkhano wacigawo , ndipo m’bale wina akumasulila m’citundu ca Cicebuano Cifukwa cake ndi loyenelela Danieli anapitiliza kukonda Mulungu na Malemba kwa moyo wake wonse . Mulungu anamva mapemphelo anga , ndipo anatithandizadi kukhala olimba mosasamala kanthu za ziyeso zimene tinakumana nazo . ” Komabe , n’navutika kusintha umoyo wanga kuti ugwilizane na mfundo za m’Baibo . Tsopano akutumikila pa Beteli . Zimenezo zinawathandiza kuti asafooke poona kuti sakupita patsogolo mofulumila . Mwacitsanzo , mtumwi Petulo ayenela kuti anali ndi nkhawa pamene anauza Yesu kuti : “ Taonani ! ( a ) N’ciani cimene Yesu analonjeza ophunzila ake ? Ena amatengela masitayelo a kudziko a kageledwe na kamangidwe ka tsitsi . Koma zindikilani kuti pothela pake , anawo afunika kucita mbali yawo kuti akulitse cikhulupililo cawo . Imeneyo idzakhala nthawi yoonetsa zimene zili mumtima mwathu . Iwo angamvetsetse mfundo yakuti kudya “ zamasamba ” kungakhale kosangalatsa ndiponso kopatsa thanzi kuposa kudya “ nyama ya ng’ombe yamphongo yodyetsedwa bwino . ” ( Miy . Kodi anacita bwanji zimenezi ? N’zolimbikitsa kudziŵa kuti tsogolo la pulaneti lathu lili m’manja mwa Mlengi wathu wacikondi , Yehova Mulungu . Kukhala anzelu ndi kumene kungatithandize kuti tikhale osiyana ndi dziko . Munthu wonyada amadziona kuti ndi wofunika kwambili , ndi kuti angacite ciliconse cimene afuna . M’banja lathu tinali kuona kuti akazi ndi otsika ndipo nthawi zambili anali kunyalanyazidwa ndi amuna . Anthu ambili amene anali padziwepo ayenela kuti anali othedwa nzelu ndi ankhawa kwambili . ( Yak . 1 : 5 ) Komanso , ngati mufufuza mosamala m’zofalitsa zathu , mudzapeza mfundo zina zabwino zimene zingakuthandizeni pa vuto lanulo . Nanga bwanji ngati mwana wanu safunabe kukambilana ? Ndipo “ Seŵelo la Eureka la Banja , ” lopenyelela ku nyumba , linali ndi mau ocepa a wosimba ndi tunyimbo . N’nali na mlongosi mmodzi cabe , dzina lake Bob . Pa lembali , cikondi cikufotokozedwa kuti ndi “ lawi la Ya . ” N’cifukwa ciani ? Ena amaona kuti n’kwabwino kulemba mndandanda wa zocitika zapadela zimene zidzacitika m’caka cimene cibwela . Kunena zoona , kupandukila Yehova n’kusaseŵenzetsa bwino ufulu wathu wodzisankhila zocita . Iwo anali atauzidwa kuti ajuŵe nthambo zingapo panthawi imodzi kuti cisalu cokhala na mau citambasuke . Pamene Yesu anali kukambilana ndi atumwi ake , anawatsimikizila mobweleza - bweleza kuti Mulungu adzayankha mapemphelo awo . — Yoh . NDI NTHAWI ITI YABWINO YOKAMBILANA NDI ANTHU ? Kodi “ mkazi wa Mwanawankhosa ” ndani ? Tingatengele bwanji cikhulupililo ca Danieli ? Tsiku loyamba limene unabwela pa nyumba yanga , ndinali nditaŵelenga Baibulo kwa maola angapo . Mofanana ndi m’nthawi ya Loti , Yehova adzawononga dziko loipali kuti athetse zoipa zimene zicitika masiku ano . 28 : 19 , 20 ) Mtumwi Paulo anazindikila kuti nchito yolalikila ni yofunika ngako . M’nthawi ya mneneli Yesaya , Yehova anayelekezela zocitika za padziko lapansi ndi mlandu m’khoti . Buku la Insight on the Scriptures , Voliyumu 2 , limakamba kuti m’Baibo , nzelu zimatanthauza “ luso loseŵenzetsa bwino zimene timadziŵa pofuna kuthetsa mavuto , kupewa ngozi , kukwanilitsa zolinga zinazake , kapena kulangiza ena mmene angacitile zimenezi . Mkwatibwi ameneyu ‘ amawelamila ’ mwamuna wake wamtsogolo ameneyu ndipo amamuona monga “ mbuye ” wake . Baibulo limatiuza kuti Miriamu , Mfumu Davide , ndi anthu ena anaonetsa cimwemwe cao mwa kuvina . ( Yoh . 13 : 3 - 15 ) Anaonetsa kuti ndi wodzicepetsa mwa kukhala womvela . Mwacitsanzo , kakambidwe kathu cabe ngakhale koonetsa mzimu uja wakuti ‘ nili na udindo wapadela ine , nimakhalako na mwayi wodziŵa nkhani zina zacinsinsi , kapena kuti nimadziŵana ndi abale amaudindo akulu - akulu ine . ’ Zoona , iye ndi “ thandizo lopezeka mosavuta pa nthawi ya masautso . ” — Sal . Koma anthu ena sanaleke kucita nkhondo ndi Asa pamodzi ndi anthu ake , mu ulamulila wake wonse . Ndipo ngati ningaganize kuti Mulungu sangateteze Baibulo , zingakhale monga nikamba kuti Mulungu alibe mphamvu . Motelo , sindinafune kuwataila nthawi mwa kuyamba kukambitsilana nao , ndiyeno mwina pakapita milungu kapena miyezi ndi kuwauzanso kuti sindifuna . Panthawiyo , tinali kutambitsa kanema yacizungu yakuti The Happiness of the New World Society . N’napita kumalo anayi othandiza anthu kuti aleke kugwilitsila nchito mankhwala osokoneza ubongo , koma sin’naleke . ( Mateyu 5 : 9 ) “ Ngati ndi kotheka , khalani mwamtendele ndi anthu onse , monga mmene mungathele . ” — Aroma 12 : 18 . Kupanduka kwa Adamu na Hava kunakhudza anthu onse mpaka masiku ano . Nsanja ya Olonda ya October 15 , 1995 , inaonetsa kufanana kwa mau a Yesu opezeka pa Mateyu 24 : 29 - 31 ( ŵelengani ) ndi opezeka pa Mateyu 25 : 31 , 32 . ( ŵelengani . ) Ndi phindu lalikulu liti limene limakhalapo ngati tipeleka ulemu woyenelela kwa amene afunikila ulemu ? Ndipo anawagwilitsilanso nchito ponena za mmene anali kudzionela . ( 1 Akor . Baibo imakamba kuti ciwombankhanga “ cimafunafuna cakudya ” kucokela pa cisa cake cimene cimakhala pamwamba pa thanthwe . Tidzaphunzila cifukwa cake Yesu anafotokoza mafanizo amenewa ndi mmene amatikhudzila . Anthu odzikondawo anali kufuna kuchuka . N’cifukwa ciani Mboni za Yehova zimayesetsa kuvala moyenelela ? Koma m’kupita kwa nthawi , Daniel anakapemphabe thandizo kwa akulu . ( Miyambo 8 : 30 ) Yesu ndiye “ Mwana wokondedwa ” wa Mulungu , komanso ni “ cifanizilo ca Mulungu wosaonekayo ” ( Akolose 1 : 13 - 15 ) Palibe amene anakhalapo pa mgwilizano wokondana kwambili monga wa Mulungu ndi Yesu . Akaidiwo anafotokoza kuti anali ndi nkhawa cifukwa cakuti analota maloto odabwitsa , koma panalibe munthu wowamasulila . Iye amatiyesa na misampha yake . Kodi Mulungu anamulonjeza ciani Danieli cokhudza tsogolo lake ? Kumbukilani kuti iye anali atauza mkazi wake kuti : “ Ndikudziŵa ndithu kuti ndiwe mkazi wokongola m’maonekedwe ako . ” Mgwilizano umene tidzafunika kukhala nao pocita zinthu zakuuzimu tingauyelekezele ndi mmene nyumba za mumzinda wa Yerusalemu wakale zinamangidwila . Makalata amene atumwi analemba analimbikitsa kwambili mipingo ya m’nthawi yawo , ndipo na ise masiku ano amatilimbikitsa ( Onani palagilafu 12 - 17 ) Yesu atalamula ophunzila ake kuti azilalikila , anakamba kuti : “ Ine ndili pamodzi ndi inu . ” Atafika anauza khamulo kuti : ‘ Conde , cokani kumahema a anthu oipawa , ndipo musakhudze cinthu cao ciliconse , kuti musaphedwe nao limodzi cifukwa ca kucimwa kwao . ’ 14 : 4 ) Nanga ndani amene adzaononga zipembedzo zimenezi zomwe zili ngati hule ? Kuyambila mu 1914 pamene “ masiku otsiliza ” anayamba , zinthu padziko lapansi zafika poipa kwambili kuposa kale . 5 : 7 Kodi Baibulo lingatithandize bwanji kulimbitsa cikhulupililo cathu ? Koma pamene cikhulupililo cathu cinayamba kukula , tinaona kuti tifunika kuwauza za colinga cathu cotumikila Yehova . ( a ) Kodi aliyense wa ife angacite ciani kuti cinyengo cisazike mizu m’mitima yathu ? A Zulu : Coyamba , umboni timaupeza mu ulosi umenewo . Izi zikanacititsa kuti asatulutse mbeu imene Mulungu analonjeza kuti idzatuluka kupitila mwa iye . — wp17.3 , peji 14 - 15 . Kumbukilani kuti Mulungu anauza Yoswa kuti : “ Buku la malamulo ili lisacoke pakamwa pako , uziliwelenga ndi kusinkhasinkha usana ndi usiku , kuti uonetsetse kuti ukutsatila zonse zolembedwamo . Pakuti ukatelo , udzakhala ndi moyo wopambana , ndipo udzacita zinthu mwanzelu . ” ( Yos . Felisa : Tsopano , ndili ndi zaka 91 . ( Aroma 14 : 21 ) Kodi mungapewe kucita zinthu zina n’colinga cakuti musakhumudwitse cikumbumtima ca ena , olo kuti muli na ufulu wocita zinthuzo ? Ndi phunzilo lanji limene tingatengepo pa zimene Yehosafati anakumana nazo ? Mwacionekele , Yehova sanafune kuchukitsa Satana mwa kuuzila atumiki ake kulemba zambili zokhudza iye na zocita zake m’Malemba Aciheberi . Koma sanapemphe thandizo kwa Yehova kapena kuyesa kudziŵa zimene anali kuganiza . 55 : 6 , 7 . Ndiyeno anamufunsanso kuti : Kodi wamulonjeza Mulungu mpemphelo kuti udzamutukila nthawi zonse ? Komabe , Yehova analonjeza kuti sadzalola atumiki ake kuyesedwa kufika pamene sangapilile , koma “ adzapeleka njila yopulumukila . ” Sukulu yapamwamba ya Shammai inamasulila lemba limeneli kuti cifukwa cimodzi cokha cothetsela cikwati ndi kucita “ codetsa , ” kutanthauza cigololo . Kodi mukanalola zimenezi kufooketsa cikhulupililo canu mpaka kuleka kutumikila Yehova ? Robert anafotokoza kuti : “ Mwana wanga atamwalila pa ngozi ya ndeke , poyamba sin’nakhulupilile . Kwa zaka zambili , adani a Ufumu “ anayambitsa mavuto mwa kupanga malamulo , ” kumenya abale athu , kuwaika m’ndende , ngakhalenso kuwapha mocita kuwamangilila , kuwaombela ndi mfuti , kapena kuwadula mitu ndi colinga cakuti asiye kulalikila . — Sal . Conco , ni bwino kufunsa kuti , Kodi umbeta wacipembedzo ni ciyenelezo ca m’Malemba ca atumiki acikhristu ? Amamvetsetsa nkhawa iliyonse imene tingakhale nayo . Akasinkhukilapo , atate wake amayamba kum’fotokozela zina ndi zina . Mu 1940 , abale athu analimbikitsidwa kuti azicita ulaliki wa mumseu tsiku limodzi mlungu uliwonse . Pa banja lathu , tinali kukonda kusonkhana ndi kupita ku nyumba ndi nyumba kukauzako ena za ciyembekezo ca m’Baibo ca tsogolo labwino . Sankhani zolinga zimene mungazikwanilitse . Mulungu adzaukitsa anyamata amene anafa kunkhondo aja , ndipo adzakhala ndi mwai wophunzila coonadi ponena za iye . Ndikauka ndimafunafuna kumene kuli madzi akuti ndisambe . Ngakhale kuti mfundo yakuti Mulungu ndi wamuyaya ndi yovuta kuimvetsa , tikhoza kuona kuti ndi yomveka . M’menemo munali kukhala dokotala wa opaleshoni , nesi wopeleka mankhwala ocepetsa ululu , ndi manesi ena aŵili amene anali kucita zonse zotheka kuti apulumutse ovulalawo . 15 : 5 ) Conco , mpesa ziimila zipatso za Ufumu zimene otsatila a Khristu amabala . 1 Tate wina ananena kuti , “ Ndikakonzekela , onse amakhala ndi phunzilo lopindulitsa . ” 1 : 12 - 14 ; 4 : 7 , 11 , 22 . Alonda amenewa amayang’anila kuti adani kapena cinthu cina cisaopseze dziko lawo . Iwo analabadila ndi mtima wonse malangizo a Yesu akuti alalikile padziko lonse lapansi uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu umene unakhazikitsidwa . Yesu anagwilitsila nchito Mau a Mulungu pokana mayeselo onse a Satana . Conco , io anazindikila kuti kuphedwa kwa Yesu ndi adani ake ndi kuukitsidwa kwake , zinali zoloseledwa kale m’Malemba . Debbie atakwatiwa , tinali ndi mwai wothela zaka 10 mu pulogalamu yomanga yapadziko lonse ku Zimbabwe , Moldova , Hungary , ndi ku Côte d’Ivoire . Koma mu 1919 , Yehova anawamasula ndipo anaonetsa bwino kwambili kusiyana pakati pa io ndi “ namsongole , ” kapena kuti Akristu onyenga . Baraki , monga munthu wa cikhulupililo anaona kufunika kopita ndi munthu woimilako Yehova , kuti iye ndi gulu lake la nkhondo alimbikitsidwe . Panthawi inayake , iye anagwilizana ndi adani a Davide poganiza kuti angapeze phindu . Onani zimene zinacitika m’nthawi ya mtumwi Paulo na mnzake Sila . Komabe , zioneka kuti Sara anasamalidwa bwino monga mlendo wolemekezeka , osati monga kapolo . 9 , 10 . ( a ) Ndi panthawi iti pamene tidzafunika kuonetsa kuleza mtima m’dziko latsopano ? Liu limeneli lingaimilenso malo amene anthu masiku ano amawaona kuti ndi opatulika , acipembedzo , kapena apadela m’njila inayake . Ni mavuto anji amene Akhristu a m’nthawi ya Atumwi anakumana nawo ? Ndipo pang’ono ndi pang’ono , mtima unakhala m’malo . ( Salimo 115 : 16 ; Tito 1 : 2 ) Ha ! N’ciani cinacitikila angelo oipawo ? 21 : 12 ) Koma kodi izi zikanatheka bwanji Abulahamu akanapha mwana wake mwa kumupeleka nsembe ? Makolo khalani abusa abwino ndipo tsogolelani ana anu modekha . Mwacitsanzo , Charles wa ku Brazil wa zaka 93 anati : “ Ukakhala ndi moyo nthawi yaitali , umakalamba . Yosimbidwa ndi Josef Mutke “ IMANI , ONANI , MVELANI . ” Ngati simungacitepo kanthu , ndiye kuti maganizo olakwika amene muli nawo okhudza munthuyo siyangasile . ( Oweruza 4 : 9 ) Mulungu anasankha kuti mkazi adzaphe munthu woipa , Sisera . Zinthu zimenezi . . . zinalembedwa kuti ziticenjeze ifeyo amene mapeto a nthawi zino atifikila . Malinga n’zimene anakamba wolemba mbili yakale wa ku Greece , dzina lake Herodotus , asilikali a Koresi anapatutsa madzi a Mtsinje wa Firate , umene unali kuzungulila mzinda wa Babulo . Patsikulo Yesu ndi ophunzila ake anacita Pasika , pokumbukila tsiku limene Yehova anapulumutsa Aisiraeli ku Iguputo zaka 1,500 m’mbuyomo . Pamene iye anafotokozela Mulungu nkhawa yake , Mulunguyo anamuuza kuti : “ Mphamvu yanga imakhala yokwanila iweyo ukakhala wofooka . ” Ngakhale n’conco , Akhiristu sali pansi pa cilamulo ca Mose ndipo safunikila kucisunga . ( Lev . Mau olimbikitsa amenewo anathandiza Rico kupitilizabe kukhala ndi makhalidwe abwino . Ndipo zimenezo zinam’thandiza kukhala paubale wabwino ndi atate wake . Nanga ni mwamuna wabwanji amene afunika kunikwatila ? ” Kodi upainiya umaphatikizapo kucita ciani ? Nanga ena mumpingo angawathandize motani apainiya ? Iwo anaona kuti munthu wotelo angawagonjetse mosavuta . ( Mateyu 10 : 11 ; Luka 8 : 1 ; Machitidwe 5 : 42 ; 20 : 20 ) Kulalikila kunyumba ndi nyumba inali njila yabwino kwambili yolalikila kwa anthu a mitundu yonse . Popeza upandu udzatha , sikudzakhalanso makampani a zacitetezo , ma alamu , apolisi , mwina ngakhale maloko ndi makiyi . 3 : 10 ) Timaonetsa ciyamikilo cathu ca mtima wonse ngati tilabadila ciitano ca Yehova cimeneci . Conco , anawalimbikitsa kugwila nchito yolalikila mwakhama , ndipo anawalonjeza kuti adzawathandiza . — Mateyu 28 : 19 , 20 . Izi zingapangitse ena kuganiza kuti mwina zimene Mdyelekezi anakamba zokhudza ulamulilo wa Mulungu n’zoona . Makolo sayenela kucitapo kanthu mwamsanga , cabe cifukwa cocititsidwa manyazi . Kodi zimenezi zikutanthauza kuti anthu amene anasiya coonadi sadzaloledwa kubwelela mumpingo ? Conco , tiyenela kutengela makhalidwe ake , ndi kuthaŵila kwa iye . 14 : 33 , 40 ) M’zaka 100 zoyambilila ndi masiku ano , Malemba athandiza gulu la Yehova la padziko lapansi kugwila nchito yofunika kwambili yolalikila uthenga wabwino . Anandiuza kuti ndipitenso ku Fort Hayes . Ndithudi , kukwatiwa “ mwa Ambuye ” n’kofunikabe . Ndiponso mwamuna wina wochuka wa mafilimu anati : “ Ndikukayikila ngati tinalengedwa kuti tizikhala ndi mkazi kapena mwamuna mmodzi moyo wathu wonse . ” Kulemekeza Yehova ndi Khristu n’kofunika kwambili . Ndipo ayenela kukhala na ciyembekezo cakuti tsiku lina mwana wosocelayo “ adzabwelela ” kwa Yehova . Yesu anati : “ Munalandila kwaulele , patsani kwaulele . ” — Mateyu 10 : 8 . Ndiyeno , anandifunsa kuti : “ Ndakalamba , ndiye ndikasiya cipembedzoci ndizicita ciani ? 4 : 11 ) Ndiyeno , akadzakonzeka adzapanga cosankha cotumikila Mulungu . 2 : 15 - 17 ; Gen . 3 : 6 ; Miy . 27 : 20 ) M’dzikoli muli zinthu zakuthupi zosiyanasiyana , zapamwamba ndi zacabe - cabe . 5 , 6 . ( a ) Kodi zinthu zinasintha motani kwa anthu a Mulungu mu Iguputo ? BUNGWE LOLAMULILA : ( Akolose 3 : ​ 14 , 19 ) Makolo abwino amakonda ndi kuyamikila ana ao monga mmene Yehova Mulungu anacitila kwa mwana wake . ​ — Ŵelengani Mateyu 3 : ​ 17 . Sakiko anati : “ Pamene tinaona kuti ali na njala yauzimu , tinayamba kuphunzila Cipwitikizi monga banja . ” 21 : 8 . Kodi Baibo Imati Ciani pa Nkhani ya Moyo na Imfa ? Na . Nyumba ya Ufumu yosamalidwa bwino imeneyi yacititsa anthu kutamanda Yehova Ndinali kufuna kuuza aliyense za iye . Patapita nthawi , ninayamba kuceza ndi banja langa uku tikuonana pa vidiyo . Izi n’zimene Ayuda akhala akukhulupilila , koma zilibe umboni . Iwo akali mu utumiki wa nthawi zonse ku Kenya . Ayenela kuti anali kudzifunsa kuti , ‘ Kodi lonjezo la Yehova lidzakwanitsidwa bwanji popeza ine sinibeleka ? ’ 23 : 8 - 12 ) Conco , n’zosadabwitsa kuti Mboni za Yehova m’mipingo yosiyana - siyana padziko lonse , zimalemekeza akulu ndi kuwakonda . Zoona , mphatso imeneyo ingakhale yamtengo wapatali , si conco ? Aisiraeli anapambana nkhondoyo monga mmene Davide anauzila Goliyati kuti : “ Yehova . . . apeleka anthu inu m’manja mwathu . ” — 1 Samueli 17 : 47 , 52 , 53 . Ena amakamba kuti zinthu zimene olosela amaseŵenzetsa ni zinthu wamba . David anandilimbikitsa kuphunzila kuyendetsa galimoto , ndipo tsiku lina ndili m’tauni ina yapafupi , ndinaona Gael . Ndinadziŵana naye pamene anali kugwila nchito m’sitolo ina ya pafupi ndi kwathu . Stéphanie ( pakati ) ( Filimoni 14 ) Zimenezi zikutikumbutsa mfundo ya pa Miyambo 12 : 24 , imene imati : “ Dzanja la anthu akhama n’limene lidzalamulile , koma dzanja laulesi lidzagwila nchito yaukapolo . ” Mkangano waukulu unabuka pakati pa alongo odzozedwa amenewa . Yehova anatipatsa ufulu wosankha zocita , ndipo ndiwo ufulu weni - weni . ( b ) Ni makhalidwe ati a Danieli amene mufuna kutengela ? Zocitika ngati zimenezi zingacititse kuti muzidziimba mlandu . Malemba amalangiza anthu amene afuna kucita cifunilo ca Mulungu kuti asamakonde dziko ndi zinthu za m’dziko . Nkhaniyo inali ya mutu wakuti : “ Kodi Nthawi za Akunja Zidzatha Liti ? ” ndipo inakamba kuti caka ca 1914 cidzakhala caka capadela . Mau a Mulungu sapeleka yankho lacindunji pa funso limeneli . Pambuyo pa milungu iŵili anabwelanso ndi anzake aŵili . Cotelo , kuyenda nawo paulendo wokaceza monga banja kungawacititse kuyamikila kwambili , ndipo kwa iwo ingakhale mphatso yabwino koposa ina iliyonse . Paulo anawayelekezela ndi thupi lopangidwa ndi ziwalo zosiyanasiyana zimene zimagwila nchito mogwilizana . Kuyambila mu 1950 , io afalitsa Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika , lathunthu kapena mbali yake cabe m’zinenelo zoposa 120 . Vuto linali lakuti iye anali kulephela kukamba . Kwa munthu wosalakwayo , limakhala vuto lalikulu . Husai sanangocita zimenezo n’colinga cakuti akwanilitse udindo wake monga nduna ya panyumba ya mfumu , koma cifukwa anali mnzake wokhulupilika wa Davide . — 2 Sam . Tikaganizila zonse zimene Yehova waticitila , kodi timafuna kucita ciani ? Ndipo inu pamwekha mufunika kutsimikiza kuti Mulungu ndiye woyeneladi kulamulila , ndi kuti ulamulilo wake ndiwo wabwino ngako . Nanga kodi abale anali kuikidwa bwanji pa udindo m’nthawi ya atumwi ? Ayuda akale anali kuopa khate limene linali lofala m’nthawi imeneyo . Cifukwa ca thandizo la Yehova , Mose anaona utumiki wake wovuta kukhala “ cuma coculuka kuposa cuma ca Iguputo . ” Ndikufunitsitsa kudziŵa zambili . N’cifukwa ciani tiyenela kusankha nthawi yabwino yokamba zinthu ? Onse akwanilitsidwa kwa inu . ( b ) N’ciani cingatithandize kuika maganizo athu pautumiki ? Iye amafuna kuti tizifuna - funa zinthu zakuthupi coyamba , pofuna kudzipezela umoyo wabwino . N’zoona kuti simupemphela n’colinga cakuti muphunzitse ana anu . Kodi kukhala wodzicepetsa kumatanthauza ciani ? Cimeneci n’cibadwa kwa mtumiki aliyense wa Mulungu . ( Ezek . 33 : 28 ; Amosi 6 : 8 ) Koma Satana amasangalala kwambili akaona anthu akuonetsa mzimu wonyada cifukwa iye ndi wonyada ndiponso wodzikuza . Yosiya anali citsanzo cabwino pankhani yolambila Yehova . 36 : 19 - 23 . Kucita zimenezi mwakhama kudzatithandiza kuti tiziona ubwenzi wathu na Yehova kukhala wofunika kwambili . 11 : 40 , 44 , 45 ; Chiv . 19 : 19 ) Ulosi wa Ezekieli umakamba kuti magulu amenewo adzabwela ngati mitambo yophimba dziko . Adzabwela na ukali kudzatiukila atakwela pa mahosi . ( Ezek . Iye anaona zotsatilapo zabwino cifukwa ca mbeu za coonadi zimene anabzala ku Lusitara . Kodi cikhulupililo cinalimbikitsa bwanji Mose pa Nyanja Yofiila ? Zonse zimene tili nazo n’zocokela kwa Yehova . Kodi kukhala anthu okhazikitsa mtendele kumalimbitsa bwanji mgwilizano ? ( Mat . 24 : 14 ) Ndipo n’nawauzanso kuti , “ Nifunika kukwanilitsa lumbilo langa kwa Mulungu . ” Ngati Adamu anapangidwa kuti adzafa , cenjezo la Mulungu likanakhala lopanda tanthauzo . Muzikhala na khalidwe labwino . ( Mat . 24 : 9 ) Komabe , ngakhale kuti timadedwa , timapitilizabe kulalikila za Ufumu ndi kukhalabe oyela pamaso pa Yehova . N’zoona kuti Mulungu angadziŵiletu za kutsogolo . Mau amenewa mulibe m’madikishonale ao , ndipo ena anali kuganiza kuti ndi dzina la malo ena ake . Mwacitsanzo , tiyelekezele kuti mukufuna kupita ku dziko lina . kudzakuthandizani bwanji kupilila pa cisautso cacikulu ? Citsanzo ca Yehova ca kudziletsa catiphunzitsa kuti nafenso tifunika kuganizila mosamala tisanakambe kapena kucita zinthu . Sitifunika kucita zinthu mopupuluma . 7 : 1 - 3 ) Aramagedo isanayambe , odzozedwa adzatengedwa kupita kumwamba . Mwacitsanzo , banja lina ku England linapempha akulu aŵili kuti akalithandize pa mavuto a m’banja lawo . Pamene muli wacinyamata ndi nthawi yabwino yopanga zosankha zofunika . Funso limeneli lagometsa mutu anthu kwa zaka masauzande ambili . Ngakhale Akhristu amene atumikila Yehova kwa nthawi yaitali , amafunika kupitiliza kukonza umoyo wawo wauzimu . — Afil . Komanso , tingawathandize kupeza kumene kuli mabungwe m’dela lathu amene angawathandize kupeza nyumba yabwino kapena nchito . Cifukwa cakuti kukambitsilana kwa conco kumathandiza banja kugwilizana ndi kulemekezana popanga zosankha zovuta . Nkhani ziŵilizi zitithandiza kuona mmene tingacitile zinthu mogwilizana ndi mapempho amenewo . * Paulo anaseŵenzetsa ufulu umene Aroma anapatsa Ayuda , poteteza Cikhiristu pamaso pa akulu - akulu a boma la Aroma . Kodi anali yekha mkazi kumeneko ? Tingaonetse bwanji kuti ndife odzicepetsa mwa mau ndi zocita zathu ? N’cifukwa ciani mufunika kukambilana zolinga zanu ndi Akhristu okhwima mwauzimu ? Kodi ananenapo kanthu koma osachita ? ” Iye anali kudela nkhawa kwambili anthu amene anali kuwaona ngati ana ake . ( Luka 10 : 1 - 12 ; Yoh . 14 : 12 ) Analonjeza otsatila ake kuti adzagwila nao nchitoyo “ mpaka m’nyengo ya mapeto a nthawi ino . ” — Mat . Patapita zaka zambili , adzukulu a Margaret aŵili , anasimbilako ana awo za cakudya ca banja cosaiŵalikaco . Anawauzanso zinthu zabwino zokhudza ambuye awo . Yehova “ anaika mzimu wake woyela mwa iye . ” Mosiyana ndi anthuwa , Mulungu amalosela ndendende zimene zidzacitika mtsogolo . Mau amene wamasalimo anakamba kuti “ Yehova wakhala Mfumu ! Inde . Zinali ndalama zokwanila kuyendela ulendo wobwelela ku dela la anthu a mtundu wa Antandiroyi na kukayamba kabizinesi kogulitsa yogati . Podzafika m’caka ca 1900 , anthu ambili anali ndi Baibulo laolao , koma sanali kulimvetsetsa . Mu 1963 , ndinaikidwa kukhala woyang’anila dela . Cifanizilo ca Agiriki kapena Aroma coonetsa mwana ali na kagalu ( pakati pa zaka za m’ma 100 B.C.E . mpaka 200 C.E . ) ( 1 Pet . 5 : 2 ) Akulu otelo saopa kuphunzitsa ena cifukwa coganiza kuti adzawalanda maudindo mumpingo . Tingatengele bwanji citsanzo ca anthu anayi amenewa ? TSAMBA 23 Mfundo ni yakuti , timakhala na cimwemwe ceni - ceni komanso umoyo wopambana , kokha ngati tiika Yehova patsogolo mu umoyo wathu . — Ŵelengani Salimo 1 : 2 , 3 . Ndiyeno wa Mboni za Yehova anafika panyumba yanga . 4 : 31 ) Cacitatu , timakonda Yehova ndi anzathu . Conco , timayesetsa kuuza ena uthenga wabwino mmene tingathele . ( Mat . Mothandizidwa ndi angelo , anali kuyang’anila nchito yolalikila , ndipo anali kudalila Mau a Mulungu popeleka malangizo . ( Genesis 2 : 24 ) Ndipo n’zosakayikitsa kuti anayesetsa kuphunzitsa ana ake za Yehova Mulungu . Kapena mukanaganiza kuti m’Baibulo muli mfundo zokwanila zoonetsa kuti nthawi zonse Yehova amacita zinthu zoyenela , ndipo iye ndiye muyezo wa cabwino ndi coipa ? ( Deut . Conco anali kupwetekedwa mtima akaganizila kuti ena a io angasiye kutumikila Yehova . “ Ukwati sudalila pa munthu mmodzi . ( Akol . 2 : 4 , 8 ) Ndiyeno , iye anafotokoza cifukwa cake maganizo ena amene anali ofala pa nthawiyo anali olakwika . Yefita ndi mwana wake anali kudalila kwambili Yehova ndipo anali kuona kuti kacitidwe kake ka zinthu ndiye koyenela . Zinamveka kuti “ akazi amasiye . . . anali kunyalanyazidwa pa kagaŵidwe ka cakudya ca tsiku ndi tsiku . ” Ambili a amene anali kudzicha Akristu , anatengela ziphunzitso zonama ndipo anakhala ampatuko . Iye amazonda anthu a “ maso odzikweza . ” Abigail anati : “ Kukamba zoona kumanithandiza kukhala na cikumbumtima coyela pamaso pa Yehova . ( Miyambo 12 : 25 ) Popeza sitingazindikile kuti Mulungu watiyankha mwa njila imeneyo , tiyenela kukhala chelu kuti tidziŵe mmene Mulungu amayankhila mapemphelo athu . N’cifukwa ciani n’kofunika kuphunzila nkhani yokhudza kukhala woyamikila ? N’ciani cina cimene tingacite kuti tikhale munthu wauzimu ? Masiku ano , Eddie amacita kulakalaka ulaliki wapoyela . Tingakhumudwe ndi kuiwala zinthu zonse zabwino zimene tingakhale nazo . ( Sal . Akhristu amenewo anali “ pa umphawi wadzaoneni , ” koma anapempha mocondelela kuti awapatse mwayi wopelekako mphatso zacifundo , ndipo anapelekadi mowolowa manja . — 2 Akor . ( 1 Petulo 4 : 7 ) Mwacidalilo timapempha Mulungu kuti atithandize , atipatse nzelu ndi kukhala olimba mtima polimbana ndi mavuto , popeza kuti “ amatimvela tikapempha ciliconse . ” — 1 Yohane 5 : 15 . Conco , tiyeni tizisinkhasinkha zimene timaŵelenga m’Baibulo kuti tidziŵe zimene amafuna . Anamwalila ali wokhulupilika pa May 13 , 2014 . Kingsley anali ndi cikhulupililo cakuti adzapitilizabe utumiki wake ali ndi mphamvu ndiponso thanzi labwino m’Paladaiso padziko lapansi . ( Yes . 35 : 5 , 6 ) — Yosimbidwa ndi Paul McManus Ndithudi , “ anasangalala cifukwa ca nsembe zaufulu zimene anapeleka , pakuti anapeleka nsembezo kwa Yehova ndi mtima wathunthu . ” — 1 Mbiri 29 : 9 . ( Aheberi 13 : 18 ) “ Wakubayo asabenso , koma agwile nchito molimbikila . ” — Aefeso 4 : 28 . Ngati tikhala olimba mtima ndi kumvela Mulungu ndi mtima wonse , ndiye kuti tikusunga lonjezo lathu . Zinali zacisoni kuti sindinapezenso mpata woceza ndi Mboni za Yehova cifukwa a m’banja langa anauza Mbonizo kuti zisakabwelenso . Conco , malinga ndi malangizo a Yesu tikhoza kuona kuti sitiyenela kuuza akulu nkhaniyo mwamsanga . Ndi nthawi iti yabwino yosinkhasinkha Malemba ? Palibe cimene tingacite kuti tikonzekele imfa ya makolo , mkazi , mwamuna kapena ya mwana wathu . Onaninso cimwemwe cimene mudzakhala naco pophunzila zambili zokhudza nyama zakuthengo m’dziko lapansi lamtendele . ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( c ) N’cifukwa ciani akulu ayenela kucita cidwi ndi nkhani ya m’Baibulo imeneyi ? 3 : 2 ) Iwo anafunika kuikabe maganizo awo pa ciyembekezo cokalandila coloŵa cawo cakumwamba . Paulo anada nkhawa kuti kulibe anamuthandiza , ndiye cifukwa cake analembela Timoteyo kuti : “ Pamene ndinali kudziteteza koyamba pa mlandu wanga , palibe amene anakhala kumbali yanga . Onse anandisiya ndekha . Mwacitsanzo , ndinayambitsa phunzilo la Baibulo locititsa coimilila kwa mwana wa sukulu wina wa pa yunivesite ku Burkina Faso , ndipo ndinauza m’bale kuti apitilize kuphunzila naye . Mau a Mulungu ali na malangizo otithandiza kupanga zosankha zolemekeza Mulungu . Atate wake anamva cisoni kwambili ndi imfa imeneyi . N’kutheka kuti inunso mwaona kuti abale ndi alongo ali ndi maluso apadela osiyanasiyana . Limodzi , aŵili , kapena ambili ? Kuwonjezela pa kuŵelenga Baibo , tifunikanso kusinkha - sinkha zimene taŵelengazo . Kodi muyenela kucita motani ngati Mkhristu mnzanu wakukhumudwitsani ? Komabe , pemphelo limene Hezekiya anapeleka linaonetsa kuti anadalila Yehova ndi mtima wake wonse kuti adzawapulumutsa . Mayankho a mafunso amenewa angatithandize kumvetsa mfundo zimene sitingazidziŵe mwamsanga . Mkazi angadandaule kuti mwamuna wake savutika kulankhula pagulu , koma amakhala cete akakhala panyumba . Pitilizani kuimbila Yehova m’mitima yanu . ” ( Akol . Kodi mungawathandize bwanji ana anu ngati simudziŵa bwino citundu cawo ? Koma kodi Mulungu amayankha bwanji mapemphelo a anthu amene amapempha citsogozo kwa iye ? Mabuku onse a m’Baibo ni ogwilizana bwino - bwino . KODI MUNGAYANKHE BWANJI ? Kodi tingagwilitsile nchito bwanji Baibulo kuti tione ngati tili ndi mtima wodzikonda ? Miyezi yoŵelengeka pambuyo potulutsidwa mu ukapolo , iwo anayamba kulakalaka zakudya na zakumwa za ku Iguputo . N’nayamba kuona Yehova kukhala weni - weni , monga tate wakuthupi wacikondi . Zimene Mulungu Wakucitilani 3 Eduardo anafotokoza kuti : “ Ndinadziŵa kuti ndinanyalanyaza ana anga makamaka panthawi imene ndinafunikila kuwasonyeza cikondi ndi kuwalangiza . MOFANANA na mtumwi Paulo , Akhristu odzozedwa na mzimu masiku ano ali na ciyembekezo cokalandila “ mphoto ya ciitano ca Mulungu copita kumwamba . ” Nditatuluka m’ndende , ndinadabwa kwambili kupeza kuti anthu 7 a m’banja langa anali kusonkhana , ndipo mmodzi wa azilongosi anga anali atabatizidwa ngakhale kuti Atate anali kuwatsutsabe . Anthu ambili adzafunafuna citetezo ku mabungwe a anthu amene ali ngati ‘ matanthwe a m’mapili . ’ ( Chiv . Zinthu zimenezi zimapweteka kwambili mtima wa Yehova . — Ŵelengani Genesis 6 : 5 , 6 ; Deuteronomo 32 : 4 , 5 . Iwo samandidula mau , samandiweluza , koma amangoti phee kumvetsela . 119 : 50 , 52 , 76 . 3 : 12 , 13 ) Mumadziŵa kuti cilangizo cimeneci n’cofunika kwambili maka - maka mukakumbukila pamene munthu wina anakuuzani mau amene anakulimbikitsani kwambili . Ophunzila a Khiristu afunika kuika Ufumu wa Mulungu patsogolo mu umoyo wawo nthawi zonse . Munthu wina wophunzitsa za cisanduliko anakamba kuti ziwalo zambili m’thupi la munthu n’zosafunika , monga kapamba . Mwa ici , iwo akanalandila “ kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . ” Koma ngati tifuna kuti Mulungu atitonthoze , tifunika kucita cinthu cina . Mkulu wa angelo , Mikayeli , ni mngelo wamkulu m’lingalilo lakuti ali ndi mphamvu na ulamulilo waukulu . Tsopano tiyeni tikambilanenso lemba la Aheberi 12 : 16 , limene limati : “ Muonetsetsenso kuti pasakhale wadama kapena aliyense wosayamikila zinthu zopatulika , ngati Esau , amene anapeleka udindo wake monga woyamba kubadwa pousinthanitsa ndi cakudya codya kamodzi kokha . ” Ngati munthu akoka fodya , nikotini amafika ku ubongo mofulumila ndi mobwelezabweleza . “ Munthu amene anali kundiphunzitsa Baibulo anali woleza mtima ndi wokoma mtima . Mwacitsanzo , mungalimbikitse apainiya ndi ofalitsa ena acangu mumpingo wanu mwa kuwauza mau olimbikitsa , kuwapatsa mphatso ina iliyonse , kapena kuwaitanila ku cakudya . Tiyeni tikambilane mmene tingapewele kulambila mafano masiku ano . ( Mac . 16 : 1 - 5 ) Akulu angatengele citsanzo ca Paulo cimeneci mwa kuyenda ndi atumiki othandiza ku maulendo aubusa ngati mpoyenela . Pambuyo pake Debora anati : “ Nyamuka , pakuti lelo ndi tsiku limene Yehova adzapeleka Sisera m’manja mwako . ( Gen . 41 : 50 - 52 ; 48 : 13 - 20 ) M’kupita kwa zaka , fuko la Efuraimu linakhala lochuka ndi lamphamvu kwambili mu ufumu wakumpoto wa Isiraeli , ndipo linayamba kuimila mafuko onse 10 a ufumuwo . Yakobo anali kukhulupilila zimene Mulungu analonjeza Abulahamu , ndipo anayesetsa kusamalila banja lake limene Yehova anasankha kuti adzaligwilitsila nchito pokwanilitsa colinga cake . ( Gen . Ngati ndife odzicepetsa , tidzaganizila mmene ena angamvelele akaona mmene tavalila . Mwacitsanzo , abale amene amathandiza Bungwe Lolamulila kukonza cakudya cauzimu , saulula kuti ndiwo amacita zimenezo . Iwo safuna kudzichukitsa . Yehova ‘ adzaletsa nkhondo mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . Apa , liu la Cigiriki lomasulidwa kuti “ umboni wooneka , ” limatanthauza “ umboni wokhutilitsa ” wa zinthu zenizeni zosaoneka . Zinthuzo zimaphatikizapo kukhalako kwa Yehova Mulungu , Yesu Khiristu , angelo , komanso zocitika za Ufumu wa kumwamba . ( Aheb . 11 : 3 ) Akazi ake ambili sanali Aisiraeli , ndipo anali kulambila mafano . Mlongo ameneyu anandithandiza kwambili kuti ndipitilize upainiya . ” Koma m’kupita kwa nthawi tinawadziŵa . Pokhala Akristu timakonda anthu , ndipo timauzako anthu ena coonadi ca mtengo wapatali . Mmene mwamuna amacitila zinthu zingathandize kuti banja likhale lolimba ndi lacimwemwe . Mosakaikila , ife tidziŵa coonadi ca m’Baibo ponena za colinga ca Mulungu cokhudza dziko lapansi ndi anthu . Tidziŵanso udindo waukulu wa Yesu Khiristu pokwanilitsa colinga ca Mulungu . ( Ezara 4 : 4 - 16 ) Mu ulamulilo wa Dariyo Woyamba ( 522 - 486 B.C.E . ) , nduna yaciperisiya dzina lake Tatenai , anapita kukafufuza za nkhaniyo . Ngati io apatsidwa zocita mu mpingo , amaona kuti ndi ofunika . N’zocititsa cidwi kuti pamene Aisiraeli anali kutumikila Yehova mokhulupilika , kuimba nyimbo inali mbali yofunika ngako pa kulambila kwawo . “ Limbitsani cikhulupililo canga ! ” — MALIKO 9 : 24 . Komanso ngati mwawaitanilako ku cakudya , sadzaiŵala mzimu wanu woceleza . Acicepele amene amaika mtima wawo wonse pa kutumikila Yehova , angakhale na cidalilo cakuti iye adzawadalitsa na kuwathandiza kukhala na umoyo wopambana . — Ŵelengani Miyambo 16 : 3 . ( Aroma 3 : 24 ; Yakobo 4 : 8 ) Mark , m’bale wa ku South Africa amene anakhala m’ndende kwa zaka zitatu cifukwa ca cikhulupililo cake , anakamba kuti : “ Kusinkhasinkha kuli ngati kupita ku malo osangalatsa . Mulungu ndiye anatilenga . Conco , Mau ake amatithandiza , kutitsitsimula , komanso kutipatsa nzelu . Iwo anamuuza kuti : “ Ngati umakonda banja lako udzapita , ngakhale kumeneko ungatumikilebe Yehova . ” Kwa miyezi , yambili m’dzikolo munali cilala cadzaoneni . Abale anaganiza kuti msonkhanowo udzaimitsidwa . ( Ŵelengani Yobu 31 : 24 - 28 ) Yobu analinso kuona kuti banja ni mgwilizano wopatulika pakati pa mwamuna na mkazi . ( Afil . 2 : 3 ) Munthu wodzicepetsa amazindikila maluso ake ndi zinthu zimene amakwanitsa kucita bwino . Cikumbumtima ni mphamvu yacibadwa imene imatithandiza kuzindikila cabwino na coipa na kutitsogolela m’njila yoyenela . Caciŵili , tiyenela kutsatila Mau ake ndi kuyesetsa kuthetsa maganizo alionse amene sakondweletsa Mulungu . Mwacitsanzo , Baibulo limayankha mafunso monga akuti : Kodi Mulungu ndani ? Mkristu amene afuna kukhala wokhwima kuuzimu amatsatila citsanzo ca Yesu , ndipo amayesetsa kumvetsetsa Baibulo mmene angathele . 2 : 19 , 20 . Ni maganizo anji amene angacititse kuti Yehova aleke kutiyanja ? Nkhani yofanana ndi imeneyi ikupezeka pa Luka 3 : 27 , pamene Salatiyeli , amene atate ake omubeleka anali a Yekoniya , akuchulidwa kuti “ mwana wa Neri . ” Iye anakamba za Mfarisi wina amene popemphela anati : “ Mulungu wanga , ndikukuyamikani cifukwa ine sindili ngati anthu enawa ayi . Iwo ndi olanda , osalungama ndi acigololo . Sindilinso ngati wokhometsa msonkho uyu . ” Koma panthawi imodzi - modziyo , wokhometsa msonkhoyo anali kupemphela modzicepetsa kwa Mulungu kuti amukhululukile . ( Onani cithunzi cili kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Kodi amakhala ndi nkhawa yotani pankhani yolela ana ? Tazindikila kuti nsembe ya dipo la Kristu ndiyo maziko a cipulumutso . Ndi mmenenso zilili ndi nchito iliyonse imene timagwila pomutumikila . Mwacitsanzo , mu 1967 pa msonkhano woyamba wa maiko ku Puerto Rico , ninavutika maganizo cifukwa ca udindo umene n’nali nawo . Kuikabe maganizo athu pa nkhani yaikulu ya ulamulilo wa Yehova kungakhale kovuta . Zimenezi zimam’kondweletsa kwambili Yehova . ( Onani ndime 20 ) ( b ) Pelekani zitsanzo zoonetsa kuti Ophunzila Baibo anali okangalika . ( Ŵelengani Salimo 84 : 11 ; Yakobo 1 : 2 - 5 . ) Iye anakana cakumwa caukali cimene cikanamucepetsela ululu koma cikanapangitsa kuti asacite zinthu mwanzelu . ( Mateyu 27 : 34 ) Yesu anaukitsidwa ndi Mulungu ndipo tsopano ali ndi moyo kumwamba . Mphatso ya dipo yocokela kwa Mulungu , imene yacititsa kuti tidzakhale na moyo wosatha , ndiye mphatso yopambana zonse 9 : 36 ) Mofanana ndi Atate ake , Yesu anali wacikondi ndi wacifundo . — Sal . Ni malemba ati amene amakutonthozani ngako inuyo ? Solomo ayenela kuti anaphunzila zambili kwa atate wake pankhani ya kulimba mtima . Olo anthu alephele kutithandiza , Yehova salephela . — Sal . Anali kudalila mzimu wa Yehova . 26 ‘ Bwelelani Mukalimbikitse Abale Anu ’ Fotokozani . ( b ) Kodi tikambilana mafunso ati ? Angakucititseni kuti mudzaonongedwe , cifukwa iye akuyembekezela cionongeko . ​ — Chivumbulutso 20 :⁠ 10 . Zimenezi zinatheka cifukwa ca dalitso la Yehova , thandizo la abale , ndiponso cifukwa ca makonzedwe amene gululi linapanga . Iwo anayamba kudandaulila Mose , ndipo vutolo linakula kwambili cakuti Mose anafuulila Yehova kuti : “ Nditani nawo anthuwa ? ( Yohane 5 : 28 , 29 ) Ponena za kuuka kwa akufa , Baibulo limatitsimikizila kuti : “ Ciyembekezo cimene tili nacoci cili ngati nangula wa miyoyo yathu ndipo n’cotsimikizika ndiponso cokhazikika . ” 103 : 8 , 19 ) Yehova ndi Mfumu yathu komanso Atate wathu wacikondi wakumwamba . Inoki atatsala pang’ono kufa , mwina Mulungu anamuonetsa masomphenya a dziko lapansi la paradaiso . N’cifukwa ciani Mose anakamba mau amenewa ? NKHANI YA PACIKUTO | KODI BAIBO IMATI CIANI PA NKHANI YA MOYO NA IMFA ? Kale , mwamuna wake anali kupita ku chalichi mwa apa ndi apo . ( 1 Akorinto 11 : 3 ) Amuna ayenela kutsogolela zocitika za m’mabanja ao . Mtsinje wa Kisoni unadzaza madzi ndi kukokolola onse ophedwa n’kukawasiya m’nyanja yaikulu . — Oweruza 4 : 16 ; 5 : 21 . 10 BAIBO IMASINTHA ANTHU Kodi ndidzatsatila mfundo zake pankhani yokhalabe ndi banja langa , ngakhale kuti zimenezo zidzacititsa kusakhala ndi zinthu zambili paumoyo ? ’ Kodi mboni ziŵili zimenezi ndani ? Popeza tinali osauka , kodi tinakwanitsa bwanji kucita zimenezi ? Kuyenela kuonetsanso kuti timayamikila kwambili cisomo ca Mulungu . Iwo anali ofunitsitsa kukondweletsa Yehova . — 1 Samueli 1 : 20 - 28 ; 2 : 26 . Mwanayo akhoza kusunga mkwiyo mumtima mwake , ndipo zimenezi zingacititse kuti asakhale paubwenzi ndi makolo ake . Tsiku lina usiku ndili woledzela kwambili , mwangozi ndinatentha nyumba yathu . 24 : 45 ; Yoh . 14 : 16 , Aroma . Tiyeni tioneko maumboni ena : M’caputala cotsatila , Yesu anagwilitsila nchito fanizo la anamwali 10 polangiza otsatila ake onse odzozedwa a m’masiku otsiliza . Koneliyo ndi a m’banja lake atalandila mzimu woyela , Petulo anati : “ Anthu awa alandila mzimu woyela monga mmenenso ife tinalandilila . Yosefe anali kudziŵa kuti Mulungu wake , Yehova , sanamuiwale ndipo mwacionekele zimenezi zinamuthandiza kupilila . Yesu anali kuonabe atumwiwo kukhala mabwenzi ake . Panthawi imeneyo ndinali ndi zaka pafupifupi ziŵili . Kodi Aisiraeli anacita ciani pamene Mulungu anawauza kuti aloŵe m’Dziko Lolonjezedwa ? Bwanji osacitako zimenezi ? ZAKA zingapo zapitazo , Cesar ndi mkazi wake Rocio , anali ndi umoyo wabwino ku California . Cesar anali kugwila nchito yolumikiza zipangizo zothandiza kuti m’nyumba muzitentha kapena muzizizila bwino . Mkazi wake Rocio anali kugwila nchito ya ganyu mu ofesi ya dokotala . Anatilandila monga mabwenzi awo ndi acibululu awo . Anatilandila bwino ku nyumba zawo . Pamene msilikaliyo anali kukambilana ndi ena , anthu aŵili osadziŵika kumene anacokela anafika pamene panali abalewo mwakacete - cete n’kuwauza kuti nawonso ni Mboni . Adolfo anati : “ Umoyo wanga unalibe colinga cililonse . Atate sanali kupeza ndalama zambili , koma anali kuonetsetsa kuti tili na pogona , zovala , na cakudya . Anali kutisamalila nthawi zonse . “ Ndinazindikila kuti sindiyenela kucita cinyengo . . . . N’cifukwa ciani n’zolimbikitsa kudziŵa kuti Mlengi wathu ndi Mwana wake amatha kulamulila mphamvu zacilengedwe ? Lomba tiyeni tikambeko za ena mwa abale na alongo amene akutumikila m’dzikoli . Sara , amene amakhala ku Colombia , anaona mmene Yehova amathandizila . Komabe , n’nali kuopa kukamba na anthu amene siniŵadziŵa . Ngati sitingacitepo kanthu , maganizo amenewa angacititse kuti tiyambe kuika patsogolo zolinga zakuthupi m’malo moika patsogolo cifunilo ca Yehova . Koma popeza kuti colinga cathu n’kukhala anthu auzimu , tiyeni lomba tikambilaneko za anthu angapo amene ni zitsanzo zabwino zoyenela kutengela . Kodi nidzakwanitsa kuzoloŵela nyengo ndi cikhalidwe ca ku maloko ? Nanga bwanji pamene zinthu zili zotivuta ? Baibo imati : “ Palibe munthu woipa aliyense amene adzamvetsetse mau amenewa , koma anthu ozindikila adzawamvetsetsa . ” Kodi sembe munamvela cisoni poona nyumba zogumuka - gumuka komanso zomela maudzu ? N’kutheka kuti anatsuka cilondaco n’kumangapo . Pamene Paulo ndi mnzake Baranaba anacilitsa munthu amene anabadwa wolemala , anthu anawatamanda kuti ndi milungu . Kodi Yehova amatithandiza bwanji ngati tayamba kuyenda njila yolakwika ? N’nali kuopa za kuphunzila citundu cina , na kuyamba kujailanso umoyo watsopano . Patapita nthawi , n’natumizidwa ku dela lina , limene linaphatikizapo cigawo conse ca Bicol . Mulungu anaona kuti cifukwa ca mtima wokonda cuma , Ahabu anakhala wopanda cifundo , cilungamo ndi cikondi . ( Luka 6 : 38 ) Khalani ndi cizoloŵezi copeza nthawi yoceza ndi ena ndi kugawana nao zinthu zimene muli nazo . M’malo mocita cabe zimene mwapemphedwa , muziyesetsa kucita mopitililapo . Kodi Agibeoni ndi Rahabi anazindikila ciani ? Limati : “ Mwana wa Mulungu [ Yesu ] anaonekela kuti aononge nchito za Mdyelekezi . ” ( 2 Akorinto 1 : 3 , 4 ) Motelo , Baibulo imatitsimikizila kuti Mulungu angakwanitse kuthandiza munthu aliyense . Conco , ngati maganizo osayenela akulepheletsani kucita zambili mu utumiki wa Mulungu , ipempheleleni nkhaniyo . ( 1 Petulo 4 : 8 ) Kukonda m’nzathu wa m’cikwati kumatithandiza kulimbitsa ukwati wathu ndi kupilila “ nsautso ” imene anthu onse amene ali pabanja amakumana nayo . — 1 Akorinto 7 : 28 . Koma ine ndinali kuona kuti Julien anali wokoma mtima kwambili , ndipo anali wofunitsitsa kuthandiza ena mu mpingo . Ngakhale kuti pangano la Abulahamu ndi pangano la Davide limatitsimikizila kuti mbeu ya mkazi idzakhala mfumu , zimenezo sizokwanila kuti mitundu yonse ya anthu idalitsidwe . Banjalo linayamikila kwambili cikondi cimeneco . Ndipo mapemphelo athu akayankhiwa , cikhulupililo cathu cimalimbilako . ( Maliko 1 : 40 , 41 ) Wakhateyo anacila . Njila imodzi imene tingawacelezele ndi mwa kuwaitanila ku cakudya . Erica anati : “ Timakondana kwambili m’banja lathu , cakuti ndinada nkhawa kuti kuyewa kunyumba kungasokoneze utumiki wanga . ” 32 : 1 , 2 ; 1 Pet . 5 : 2 - 4 ) Conco , mkulu wacifundo samalamulila abale ndi alongo , kupanga malamulo , kapena kuwapangitsa kudzimva kuti ali ndi mlandu mwa kuwakakamiza kucita zimene io sangakwanitse . Cinthu coyamba n’cakuti , zakumwamba zimaonetsa mphamvu za Mulungu . Nikumbukila kuti tsiku lina , iwo ananionetsa Baibo na tumabuku twina twa m’citundu ca Citagalogi tovumbula ziphunzitso zabodza za cipembedzo . Ngakhale kuti tikukumana ndi mavuto , tingacite ciani kuti tipitilize kukonda abale athu ? Nthawi zonse , gulu la Yehova limatipatsa malangizo othandiza kuongolela ulaliki wathu . Tiyenelanso kudziŵitsa akulu mwamsanga kuti amupatse thandizo loyenelela . N’ciani cimene taphunzila m’mafanizo atatu awa ? TSAMBA 6 • NYIMBO : 92 , 120 M’malo momukalipila , m’baleyo anangotenga mapaketiwo n’kuwaika pamalo ake . Ayuda ambili sanalandile uthenga wabwino ndipo anakumana ndi mavuto . Yesu anacenjeza ophunzila ake kuti : “ Mukadzaona magulu ankhondo atazungulila Yerusalemu , mudzadziŵe kuti cionongeko cake cayandikila . N’tamvetsetsa tanthauzo la masomphenya amenewo , n’nadziŵa cifukwa cake okwelapo ake akufotokozedwa mwa njila imeneyi . ” — Ed . “ Kapolo sangatumikile ambuye aŵili . . . . KHULUPILILANI KUTI YEHOVA AMATIMVELA Komabe , mmishonale wina amene watumikila kumeneko kwa nthawi yaitali anawauza kuti : “ Zimene muyenela kudziŵa n’zakuti kungopatsa munthu kapepala kauthenga , mwina zingakhale kuti munthuyo ndi nthawi yake yoyamba kumva uthenga wa Yehova . Conco , kuti tikwanitse kupewa mtima wodzikonda , coyamba tiyenela kuŵelenga Mau a Mulungu mosamalitsa . Pocezela mipingo yosiyana - siyana m’dela , n’nali kupeleka nkhani m’tumakhumbi twaudzu , m’mitsika , pamabwalo a maholo a khanso , pamabwalo a maseŵela , m’mapaki , ndipo nthawi zambili m’makwalala . Yesu sanali cabe Mbuye kwa atumwi ake . Baibo imakamba kuti Sara “ anali wosabeleka , conco analibe mwana . ” Davide anakamba kuti : “ Yehova ndiye mwini nkhondo . ” — 1 Samueli 17 : 45 - 47 . Pangatenge nthawi kuti tidziŵe ulemu woyenelela umene tiyenela kupeleka kwa ena ndi mmene tingaupelekele . Amene analemba Salimo 104 anayamikila kwambili Yehova cifukwa ca zinthu zonse zimene analenga moti analemba nyimbo yomutamanda . Anthu okhulupilika amenewa anasankha kukhala ku mbali ya Yehova , komanso anadzipatula kwa anthu ocita zoipa . Lekani nifotokoze cifukwa cake ine na mkazi wanga Maria , tinali okonzeka ‘ kuvutika cifukwa ca cilungamo , ’ ndi mmene tinadalitsidwila cifukwa cokhalabe wokhulupilika . — 1 Pet . Nthawi zina Yehova amalola zimenezi kucitika . Kaya acite kukamba zimenezi kapena ayi , iwo angamvele ngati Davide amene anati : “ Udalitsike cifukwa ca kulingalila bwino kwako . ” Conco , ngati munthu wina watikhumudwitsa , tiyenela kuganizila zimene Yehova amafuna . Komabe , wamasalimo anapitiliza kutamanda Yehova . Mukamaona zocita za mbalame , muziyesanso kukumbukila zimene Malemba amakamba zokhudza mbalamezo . ( b ) Kodi mtumwi Paulo anaonetsa kuti n’ciani cina cimene cingatilimbikitse ? Munthu amene apatsidwa malangizo mwanjila imeneyo angaone ‘ kukoma ’ kwa mau othandiza amenewo . Kodi pa Oweruza 5 : 20 , 21 pamafotokoza mfundo zina ziti zokhudza nkhondo yolimbana ndi Sisera ? Nthawi zina , anali kusintha mau a m’Baibulo kuti agwilizane ndi zikhulupililo zawo , m’malo mokhulupilila zimene Baibulo imaphunzitsa . 8 : 9 ) Ndiyeno , analangiza aja amene anali na cikumbumtima cofooka kuti sayenela kuweluza anzawo amene anali kudya nyama imeneyo . Pa zaka zonsezi , Mfumu yathu Yesu Kristu , yakhala ikutsogolela nchito yolalikila . N’cifukwa ciani anaganiza zosiya kukoka fodya ? Iye anayamba kulamulila mu 1914 , ndipo posacedwa adzatsiliza kugonjetsa mwa kuthetsa mavuto onse . Apa n’zoonekelatu kuti kusunga cuma kapena zinthu za kuthupi sikungatipulumutse . Kora , Datani , na Abiramu anayamba kutsutsana na Mose cifukwa ca nsanje . Nanga anagwila nchitoyi n’ndani ? Mwacitsanzo , Yeremiya analosela kuti mzinda wa Yuda udzaonongedwa ndi Ababulo , ndipo zimenezo zinacitikadi mu 607 B.C.E . M’zaka zambili zimenezo , atsogoleli a machalichi ndiponso olamulila andale anali kufuna kumalamulila anthu . M’mbuyomo , iye anali atabatizikapo kale m’zipembedzo zosiyana - siyana . N’nali kukhala m’nyumba ya amishonale ku Asunción , pamodzi na mnzanga wina wake . 21 : 3 , 15 ; 2 Mbiri 24 : 20 , 21 ) Danieli na anzake anali na ufulu wosankha kusiya cikhulupililo cawo kuti amasulidwe . Tiyeni tikambilane zocitika zitatu zoonetsa kupanda cilungamo kumene kunacitika pakati pa anthu a Yehova m’nthawi yakale . Kuti tipambane polimbana ndi Satana , tiyenela kuona zinthu za kuthupi m’njila yoyenela . — Ŵelengani 1 Timoteyo 6 : 6 - 10 . Popeza n’nali na zaka 5 cabe , n’nacita mantha . 3 : 14 ) Conco , mosasamala kanthu ndi zilizonse , Yehova adzakhala ciliconse cofunikila kuti akwanilitse cifunilo cake . Ambili amapeleka mayankho oonetsa kuti ali na zolinga zimene afuna kudzakwanilitsa potumikila Yehova , monga kuyamba utumiki winawake wa nthawi zonse , kapena kukatumikila kumene kuli ofalitsa Ufumu ocepa . Paulo analemba kuti : “ Tikugonjetsa zinthu zonsezi kudzela mwa iye amene anatikonda . Timayamikila kwambili Yehova cifukwa copanga makonzedwe akuti zikhale zotheka kukhala mabwenzi ake ngakhale kuti ndife opanda ungwilo . — Ŵelengani 1 Timoteyo 1 : 15 . Kodi ena a maudindo amene ali nawo pali pano , angafunikile kusiila abale ena kuti asamalile bwino udindo watsopano ? Zikuoneka kuti ngamila zimenezo zinali ndi ludzu kwambili . Mwacitsanzo , Ophunzila Baibulo m’dziko la Germany anapatsidwa milandu yambili cifukwa colalikila . Ganizilani kuti muyenda m’mbali mwa mtsinje , ndipo mwaona kanthu kena kooneka ngati kamwala kakang’ono konyezimila . Akatswili ofukula zinthu zakale atalumikiza mapalewo bwino - bwino , anakwanitsa kuŵelenga mawuwo . Ngati ndinu Mkristu wodzozedwa , ciyembekezo canu ca kumwamba ndi nkhani imene muyenela kuipemphelela nthawi zonse . Ndi mavuto otani amene omasulila akumana nao pomasulila Baibulo la Dziko Latsopano m’zinenelo zina ? Omasulila ena amakamba kuti cifukwa cimodzi cocitila zimenezi n’cakuti , dzina lenileni la Mulungu limene limaimilidwa na zilembo zochedwa Tetragalamatoni ( YHWH ) , silionekela olo pang’ono m’Baibo ya Cigiriki ya Septuagint imene inamasulidwa kucoka m’Malemba a Ciheberi . Kuti timvetsetse mmene tifunika kucitila zinthu na Akhristu anzathu mumpingo , ganizilani izi : M’nthawi ya Aisiraeli , ziwiya za m’kacisi wa Yehova zinali kukhala zopatulika . Timaonetsa kuti tifuna kuyandikila Yehova ndi Mwana wake . Cifukwa cakuti kupewa mtima umenewu kudzatithandiza kukhala ndi cikondi cacikristu , khalidwe limene ophunzila a Yesu amadziŵika nalo . N’tatulutsidwa m’cipatala , n’nayambanso kuyenda kusukulu . Ngakhale kuti umoyo ndi mautumiki athu asintha , ubwenzi wathu sunasinthe . ” Nili na zaka 7 , n’natumizidwa ku sukulu yophunzitsa za cipembedzo . Zoonadi , kuti ubatizo ukhale woyenelela , coyamba munthu afunika kudziŵa cifunilo ca Yehova molondola . ( 2 Mbiri 11 : 3 , 4 ; 12 : 6 ) M’kupita kwa nthawi , iye anayambanso kucita zoipa . Mosiyana ndi bodza limene Mdyelekezi anakamba , Yehova samana olambila ake okhulupilika zinthu zilizonse zabwino . Pamenepo Yaeli anaonetsa Baraki mtembo wa Sisera cikhomo cili m’mutu mwa Siserayo , ndipo Baraki anazindikila kuti ulosi umene Debora anakamba wakwanilitsidwa . Tidzakambilana mafunso amenewa m’nkhani yotsatila . 19 : 33 , 34 . Ndiyeno anapitiliza kuti , “ Ngati umandikonda udzandiuza . ” Kodi ‘ mumamvetsetsa ciliconse ’ cofunikila kuti mukwanitse kukondweletsa Yehova ? 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani n’cinthu canzelu kukhala ku mbali ya Yehova ? Koma pamene mufika pa sitesheni ya basi , mupeza kuti pali mabasi yambili na cigulu ca anthu a paulendo . Mphatso yokhala pa ubwenzi na Yesu . Afunseni za umoyo wawo na mmene utumiki ukuyendela . — Miy . “ Iye adzapukuta misozi yonse m’maso mwao , ndipo imfa sidzakhalaponso . ” — Chivumbulutso 21 : 4 . Ndiye cifukwa cake zolemba zambili zakale kulibe masiku ano . Mtumwi Paulo anafotoza zinthu zina zimene zingatithandize kukhala ndi maganizo oyenela . Caka cotsatila , tinauzidwa kukatumikila ku Kampala ku dziko la Uganda , ndipo tinali amishonale oyamba kumeneko . ( a ) N’cifukwa ciani tiyenela kusankha bwino mau okamba ? 6 : 7 , 8 . 12 : 2 ) Panalibe mtsogoleli wina anaonetsapo umboni wotsimikiza umenewu . Masiku ano , caka ciliconse Cipilala ca Tito cimacititsa cidwi anthu masauzande ambili amene amapita kukaona malo ku Rome . Regina wa ku Philippines anafotokoza mavuto osiyanasiyana amene anakumana nao . Mavuto monga kupezela banja lake zinthu zofunika pambuyo pa imfa ya mwamuna wake , kucotsedwa nchito , ndi kulela ana . wankhanza ? Lomba nili na zolinga zatsopano pa umoyo . ” Ndipo anthu 30 sauzande anapempha mabuku ofotokoza Baibulo . M’madela ena , cinthu cimene cimavuta n’cakuti makolo amene si Mboni amafuna ndalama zambili za malowolo , moti abale osauka zimawavuta kukwatila . 8 Thandizo pa Kupewa Mavuto M’bale wina amene anaikidwa kukhala woyang’anila watsopano wa dipatimenti ina pa msonkhano , anatumila foni m’bale wina ndi kum’pempha ngati angakonde kutumikila m’dipatimenti imeneyo . Nanga analiona bwanji khalidwe lawo la kuona mtima ? N’cifukwa ciani tiyenela kucita cidwi ndi zidutswa zopezeka pa zinyalala zakale za ku Iguputo ? 1 : 3 - 5 . Tsiku lina pamene tinayenda kukaona malo osungila zinthu zakale ochedwa British Museum , M’bale Schroeder anatilatila mipukutu yakale ya Baibo . Kamasulidwe katsopanoka n’kogwilizana bwino na mavesi ena a m’salimoyi . Conco , tiyenela kuphunzila n’colinga cakuti ‘ tidziŵe ’ bwino Yehova osati kuti tidziŵe cabe zinthu zatsopano . — Ŵelengani Ekisodo 33 : 13 ; Sal . Kapena pamene munali kumvetsela mwachelu mnzanu pokukhutulilani zakukhosi kwake ? ( b ) Kodi Yesu anali kumuona bwanji kacisi wa Mulungu ku Yerusalemu ? Iwo atengeka ndi zaciwelewele , ndipo pa cifukwa cimeneci akumana ndi zowawa . Kodi izi zinacitika cifukwa cakuti Mulungu anaona kuti tikhoza kupilila ? ’ 13 : 11 . Kodi muyenela kusamala za ciani pamene mufuna - funa nchito ? Iye ndi “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse . ” — 2 Akorinto 1 : 3 . Timaonetsa kuti tili ndi cikhulupililo tikamapilila mavuto amene tikumana nao ( Onani ndime 14 ) Kucita zimenezi kudzatithandiza kuti “ tisakwiyile Yehova . ” — Ŵelengani Miyambo 19 : 3 . ( Luka 1 : 31 , 35 ) Conco , Yesu anali munthu wangwilo , monga mmene Adamu analili atalengedwa . Ngakhale zinali conco , ndinasankha kusiya masewela a zibakela kuti ndiyambe kuphunzila Baibulo . Koma abale anga sanasangalale ndi zimenezo . ( Ŵelengani Agalatiya 4 : 17 ) Anthu ena mumpingo anafuna kupangila anzawo zosankha pa nkhani zaumwini ndi colinga cowapatutsa kwa atumwi . Potengela citsanzo ca Atate wathu wakumwamba amene ndi wacifundo , woleza mtima ndi wacikondi , nthawi zina tingaone kuti tifunika kusintha maganizo athu . Komabe , Mulungu ‘ sanatimane Mwana wake wa iye yekha . ’ 5 : 3 ; Afil . M’maiko ambili mukali kufunika a nchito ambili okolola mwa kuuzimu . Koma adani athu adzakhumudwa kwambili ndi uthengawo . Timadziŵika ndi nchito yolalikila kunyumba ndi nyumba , pamalo amene pamapezeka anthu ambili ndi kulikonse kumene tapeza anthu . Iye anacita mantha . Ngati mpingo uliwonse watsopano wakhala ndi akulu 5 , ndiye kuti atumiki othandiza 10,000 angafunike kuyamikilidwa caka ciliconse kuti akhale akulu . Ciŵelengelo cimeneci cikuonetsa kuti dzina la Mulungu lachulidwanso m’mavesi ena 6 kuonjezela pa ciŵelengelo cakale . Caka ca 607 B.C.E . cisanafike , Yehova anaonetsa Ezekieli masomphenya a zimene zidzacitika m’Yerusalemu , mzindawo utatsala pang’ono kuonongeka . N’zacidziŵikile kuti ufulu umene Yesu analonjeza ophunzila ake ni weni - weni . Sungalingane na ufulu wa zacikhalidwe kapena wa zandale umene anthu ambili amaulakalaka masiku ano . Iye anakamba kuti : “ N’nali kudziona monga munthu wacabe - cabe , koma nikapempha Yehova kuti anikhululukile , anali kunithandiza . ” Mtumwi Paulo analimbikitsa kukhala mbeta . Komabe anati : “ Cifukwa ca kuwanda kwa dama , mwamuna aliyense akhale ndi mkazi wake - wake ndipo mkazi aliyense akhale ndi mwamuna wake - wake . ” M’kupita kwa nthawi , anacokako cifukwa cokhumudwa ndi zocitika za kumeneko . Ndili ndi zaka 14 , ananditumiza kusukulu ya boding’i ku Germany . Mkulu wina , mkazi wake na ana ake , anangonitenga monga wa m’banja mwawo weni - weni . “ Mphamvu yoposa yacibadwa ” imacokela kwa Mulungu , osati kwa ife . — 2 Akor . Ponena za Mlengi wathu , Yehova Mulungu , * Baibo imati : “ Ciliconse iye anacipanga cokongola pa nthawi yake . Ngakhale pambuyo pa zaka zambili , abale ndi alongo saiwala kuti m’bale Pierce anali kukonda kuceleza , anali waubwenzi , ndipo anali kukonda kulimbikitsa ena pogwilitsila nchito Malemba . Nkhondo imeneyi ndi umboni wosatsutsika wakuti Satana anathamangitsidwa kumwamba . Monga taonela m’nkhani yapita , Mulungu adzathetsa kuvutika ndi kupondelezana kumene kwakhalapo kwa zaka zambili . Kodi Yesu anacita ciani ? Kodi kuona zabwino mwa ena kudzatithandiza bwanji ? Nanga kodi nimawaseŵenzetsa ? ( Neh . 9 : 20 , 21 ) Kupitila mwa mneneli Elisa , Yehova mozizwitsa anaculukitsa mafuta ocepa amene mayi wina wamasiye wokhulupilika anali nawo . Mofanana ndi Paulo , atumiki ena a Yehova masiku ano asankha kusaloŵa m’banja , n’colinga cakuti acite zambili mu utumiki wa Yehova . Mobwelezabweleza , io anaphwanya malamulo a Mulungu . ( Yakobo 2 : 18 ) Zocita zathu zimaonetsa ngati tili ndi cikhulupililo colimba . Tingaonetse bwanji kuti tikucilikiza ulamulilo wa Mulungu ? Conco , tisagonje cifukwa tili pankhondo ya kuuzimu yomenyela cikhulupililo cathu . Tsiku lina , anzanga a ku nchito anayamba kunionetsa zamalisece . NYIMBO : 120 , 64 Kodi kalata ya Yohane inam’limbikitsa Gayo kupitiliza kuceleza alendo ? Pambuyo podutsa m’cipululu , Aisiraeli anafika ku Refidimu kumene kunali kufupi ndi Phili la Sinai . 7 : 12 . ( Yobu 29 : 7 - 16 ) Ngakhale zinali conco , iye sanayambe kudzikweza , kapena kuleka kudalila Mulungu . Poseŵenza ndi ena , khalani woganizila ena ndi waulemu ndipo yesetsani kuwayamikila na kuwalimbikitsa . Conco , n’kofunika kuti tizikonda Yehova ndi mtima wathu wonse . ( Maliko 12 : 31 ) Ngati timadzizonda ise eni , n’zosatheka kukonda anzathu . ( Aheberi 5 : 7 ) Zitsanzo zina timazipeza pa Danieli 9 : 21 ndi 2 Mbiri 7 : 1 . ( Yohane 1 : 14 , 17 ; Akolose 1 : 15 ) Mtumwi Paulo anakamba kuti angelo naonso amakambilana m’cinenelo cosiyana kwambili ndi ca anthu . — 1 Akorinto 13 : 1 . Iye anati : “ Ndikakwiya , sindimacitapo kanthu nthawi imeneyo . Ndimayembekezela nthawi yabwino yakuti tikambilane za vutolo ndi kuona mmene tingalithetsele . ” Ndikupita mu ulaliki ndi Demetrius Papageorge , m’bale wodzozedwa amene anayamba kutumikila Yehova mu 1913 12 : 7 - 9 . Mwacitsanzo , pankhani yocita Pasika caka ciliconse , anthuwo anauzidwa kuti : “ Ana anu akadzakufunsani kuti , ‘ Kodi mwambo umenewu umatanthauza ciani ? ’ [ Mau apansi ] M’maiko ena makolo amakhala pamodzi ndi ana ao aakulu ndipo mabanja ena angasankhe kucita zimenezo . Tinali kulalikila m’gawo limene linali pamsenga wa makilomita 16 mpaka 24 , kucokela pamene tinaika kalavani yathu . Tingaphunzile ciani pa nkhani ya Aroni ndi imfa ya ana ake ? Cinsinsi Namba 6 Cilango Koma sitisonkhetsa ndalama , kapena kulipilitsa anthu ndalama ndipo mabuku athu sitigulitsa . ( Luka 12 : 48 ) M’mbuyomo , Yehova anaweluza mtundu wonse wa Isiraeli kuti sudzaloŵa m’dziko la Kanani cifukwa ca kupanduka kwawo . Inde , tidzakhalanso omasuka kulalikila tikapeza mpata . Kucita izi kumawathandiza kupanga ubwenzi na abale a kudzikolo , ndiponso kumawathandiza kuti ajaile cikhalidwe catsopano . Iye anakamba mau amenewa malinga ndi zimene zinam’citikila . Pasanapite nthawi , anthu ambili anayamba kucita cidwi ndi coonadi . 30 Za M’nkhokwe Yathu Kodi zosankha zanga zidzanithandiza ndi ‘ kukhala mwamtendele ’ ndi ena ? Mofanana ndi akazi ambili a m’nthawiyo , Rabeka anali ndi nchito zambili zogwila , monga kutunga madzi a banja lonse . Yelekezani kuti mukuona Sara m’nyumba yacifumu akuyang’ana pawindo kuona dziko lokongola la Iguputo . 71 : 5 . Mau a Mulungu amatiuza mmene tingapewele ciwelewele . Tinacita kuchula deti imene tinali kufuna kuyenda kumeneko . ” Makalatawa amanilimbikitsa kwambili . Napindulanso ngako na cilimbikitso cocokela kwa Dennis mng’ono wake wa Arthur , mkazi wake , komanso Ruth na Judy , ana a mlongosi wanga . Iye anaonetsanso cikondi copanda dyela mwa kupatsa Adamu na Hava ciyembekezo cokhala na moyo wosatha m’Paradaiso amene anawakonzela . ( Oweruza 11 : 30 , 31 ) Kodi zimenezi zinali kutanthauza ciani ? Makhalidwe ena abwino ofunika . Ngati mukufuna wokwatilana naye , n’ciani cimene mungaphunzile kucokela kwa Msulami ? Iye anapitiliza kuti , Yehova “ amatumiza mau ake ndi kusungunula madzi oundanawo . ” Kodi cinali ciani ? PA March 31 , 2018 , pamene dzuŵa lizikaloŵa , anthu a Mulungu na okondwelela ambili adzasonkhana pa Mgonelo wa Ambuye , umene umacitika kamodzi pa caka . Koma popeza io “ anacoka pakati pathu , ” anapatuka pa ziphunzitso zolondola za m’Baibulo . Yehova adziŵa bwino - bwino tsiku limene cisautso cacikulu cidzayamba cifukwa anacita kusankhilatu tsikulo . Mbali zonsezi zingathandize acicepele ndi acatsopano kuti aphunzile kuthandiza ena . Conco , kukulitsa cikondi pa Yehova komanso kudana ndi zoipa ndiye cisinsi cothetsela vuto la kutamba zamalisece . — Ŵelengani Salimo 97 : 10 . Pamene anali kumeneko , mzimu woyela mobweleza - bweleza unamuletsa kulalikila m’madela ena m’cigawoco . “ Mulungu . . . acititse nonsenu kukhala ndi maganizo amene Khristu Yesu anali nawo . ” — AROMA 15 : 5 . Conco , sitiyenela kuganiza kuti anthu ena sangamvetsele uthenga wa Ufumu . Mboni za Yehova zoposa 7,500,000 ‘ zam’pezadi ’ ndipo zimam’konda kwambili . ZIMENE KUKONDA MULUNGU KUMATANTHAUZA ( 2 Tim . 1 : 5 ; 3 : 14 , 15 ) Pamene anali na zaka pafupi - fupi 20 kapena kuposelapo , Timoteyo anali atakhala Mkhristu wofikapo , woti n’kupatsidwa maudindo apadela mumpingo . — Mac . 10 , 11 . ( a ) N’cifukwa ciani tingakambe kuti pemphelo ndi mwai wamtengo wapatali wocokela kwa Yehova ? Komabe , kuti tiyandikile Yehova , tifunika kuphunzila ndi colinga coyenela . 4 : 9 , 10 ) M’lingalilo leni - leni , Yesu analoŵa m’malo atate wathu waumunthu woyambilila , Adamu . Anali kucita “ cilungamo ” kuti anthu aŵaone . Davide anakumana ndi mkazi ameneyu panthawi imene anali kuthaŵa Mfumu Sauli . Yehova ndi Akristu anzanu samaiŵala zimene mumacita pom’tumikila . — Ŵelengani Malaki 3 : 16 ; Aheberi 6 : 10 . ( Chiv . Mmene Mulungu Amatitonthozela 4 Koma mwamunayo akacokapo , zingakhale zovuta kum’lemekeza . Zinthu zikakhala telo , anthu oona mtima ndi amene amavutika kwambili . ( Yobu 6 : 3 ) Ndithudi , n’zomveka kuti anamva conco . Nanga n’ciani cinacititsa kuti maganizo akuti Cilamulo ca Mulungu cimavomeleza kubwezela ? Zimenezi zingapangitse kuti cikhale covuta kwa makolowo kuphunzitsa ana awo mfundo zozama za ‘ m’malemba oyela . ’ ( 2 Tim . Mwacidule , taona kuti kutulila Mulungu nkhawa zathu m’pemphelo locokela pansi pa mtima , kuŵelenga Mau ake , ndi kusinkha - sinkha n’zothandiza kwambili . Ndi nchito yotani imene Yehova anapatsa Mose ? Nanga anam’tsimikizila za ciani ? Woyang’anila ndende wa kumeneko anakondwela kuona kuti ndabwela , ndipo anafuna kuti ndikhale “ mbusa ” pandendepo . M’masukulu a boma munali kucitika miyambo yosonyeza kukonda dziko , monga kucitila sawacha mbendela ndi kuimba nyimbo ya fuko . N’ciani cimene Mariya anacita cimene Yesu anayamikila ? Kukatsala mawiki ocepa kuti ticite Cikumbutso , iye amaŵelenganso nkhani zimenezo ndi kusinkha - sinkha kufunika kwa mwambo umenewu . ( 1Tim . 1 : 19 ) Mungacite bwino kupewa nchito imene ingaononge ubwenzi wanu ndi Mulungu . — Miy . Kodi anangokhala cete n’kuyembekezela kuti munthu wina adzapita kwa mfumu kukakamba nayo za colakwa cake ? Satana anakamba kuti Mulungu anali kuŵamana cinthu cina cabwino , cimene ni ufulu wodzisankhila cabwino na coipa . Iwo anasankha kukhala kumbali ya Satana na kupandukila Mulungu . 11 , 12 . ( a ) N’ciani cingatithandize kuona zofooka za anthu moyenela ? Lemba limenelo limanenanso kuti anatsatila mosamalitsa zimene anauzidwa . Tsiku lotsatila , mkulu wa apolisi ananditenga ndi kupita nane ku cipinda cina , kumene analemba cikalata cimene cinali ndi mau akuti : “ Ine Trophim R . ( Salimo 34 : 8 ; Miyambo 10 : 22 ) Pamene tikuphunzila zambili zokhudza Mulungu ndi kuona mmene akutithandizila , ubwenzi wathu ndi iye umalimba kwambili . Onani kuti pempho laumwini limeneli silikukamba kuti cakudya “ canga ” calelo koma likuti cakudya “ cathu ” calelo . Pa usiku umodzi , Blessing anafunika kupanga ndalama pafupi - fupi madola 200 mpaka 300 a ku America . Cinthu cimodzi cofunika kwambili cimene cingatithandize kupilila mayeselo ndi kupemphela kwa Yehova kuti atithandize . N’cimodzi - modzi masiku ano . Anthu ena amene poyamba sanali kulabadila uthenga wathu wa m’Baibo , angayambe kumvetsela na kusakila thandizo pambuyo pokumana ndi mavuto aakulu mosayembekezeleka . 1 ) Inde , ngakhale pamene anakumana ndi mavuto aakulu , iye anapitiliza kukonda Mulungu . Tingatengenso phunzilo lina ku banja limene Yosefe anali kucokela . Komabe , n’kutheka kuti pamene muiŵelenga mudzakhala na mafunso ambili . Cifukwa ca thandizo la Yehova , ndilinso pa ubwenzi ndi Amai . Koma kutumikila Yehova kwanibweletsela cimwemwe cacikulu , ndipo nimakhala okhutila na zimene nacita . ” Satana ndiye “ tate wake wa bodza . ” Mwina inunso mumawaona akulalikila kunyumba ndi nyumba kapena kumalo ena amene kumapezeka anthu ambili , akugaŵila mabuku ofotokoza Baibulo mwina akucititsa phunzilo la Baibulo kwaulele . Mwa kutelo , cikhulupililo canu cidzakhala colimba mwa Mulungu . Mabuku ena ofufuzila amafotokozanso mfundo imeneyi , koma si akatswili onse amene amavomeleza zimenezi . Tiyeni tikambilane mfundo zitatu zimene tingaphunzilepo . Anatelo n’colinga cakuti anthu aŵelenge uthenga wonse , osati mbali zocepa cabe . 134 - 136 . Jérôme , mmishonale wa ku French Guiana , wathandiza acicepele ambili kukhala amishonale . Tiyeni tikambilane zitsanzo za acinyamata ena zimene Akristu acinyamata angatengele . DZIŴANI kuti muli pankhondo . 6 : 1 ) Kumatipatsa mwayi ‘ wokana moyo wosaopa Mulungu ndi zilakolako za dziko . ’ ( Miyambo 15 : 17 ) Pali mfundo yanji ? Kodi tidzaonetsa kuti timawakonda ? Paulo anafotokoza amene anali woyenelela kulandila cithandizo mumpingo . Ndipo kunena zoona nthawi sibwelela m’mbuyo . ” 28 : 5 ) Ifenso tingathe kutengela citsanzo cawo . Ngati mumalephela kudziletsa pa kamwedwe ka mowa , muyenela kupewa zocitika zimene zingakuikeni pa ciyeso cakuti mumwe kwambili . Ndinafunika kukhala woleza mtima . Mofananamo , ngati mudziŵa bwino zolinga zanu mu umoyo , kupanga zosankha mwanzelu sikukhala kovuta . Mbali imodzi inali kuchedwa kuti Tsidya la Mtsinje , ndipo inaphatikizapo Kole - Suriya , Foinike , Samariya , ndi Yuda . Motelo , bukuli linasankhidwa cifukwa cakuti limafotokoza za banja limene Yesu anabadwilamo , ulaliki wake wochuka wa pa phili , komanso ulosi wocititsa cidwi wokhudza masiku otsiliza . Anthu a ku Japan amacita cidwi ndi nkhani zimenezi . Iwo anazindikila kuti ndinali kufuna kumvetsetsa Baibulo ngakhale ndinali kukamba kuti sindikonda za cipembedzo . Koma Cilamulo ca Mose cinakamba kuti aliyense wogwila mtembo anali wodetsedwa . ( Eks . 12 : 38 ) Kodi zikanakhala zanzelu ngati Aisiraeli ena , mwina acinyamata , akanapanga kagulu n’kuyamba kuyenda njila imene io akanaona kukhala yoyenela ? Koma popeza kuti tsopano ali m’ndende , iye alibenso ufulu woyenda . Timaona nyumba yathu kukhala yofunika kwambili , ndipo timafuna kuti ena aziilemekeza . Iye anati : “ Tinalephela kupeleka cisamalilo ca nthawi zonse cimene amai anali kufunikila . Kuti apeleke yankho , Mulungu walola kuti anthu adzilamulile kwa kanthawi . 24 : 14 ; Afil . 2 : 15 ) Zimenezi zathandiza anthu ambili kuti akhale olungama pamaso pa Yehova . — Ŵelengani Danieli 12 : 3 . Kutsatila malamulo a Mulungu na mfundo zake , ‘ kumabwezeletsa moyo , kumasangalatsa mtima , komanso kumatsegula maso . ’ — Salimo 19 : 7 , 8 . Satana anayambitsa mkangano mu Edeni pamene anatsutsa ulamulilo wa Yehova . 4 : 17 ) Mau acidule amenewa aonetsa kuti panali mgwilizano wamphamvu pakati pa Paulo na Timoteyo . Yakobo na Rakele ? Munali kumva bwanji pamene tinali kuphunzila makhalidwe a Yehova ? Nanga munali kumva bwanji pamene munali kumvetsela ndemanga za Akristu anzanu zoonetsa mmene amakondela Yehova ? Koposa zonse , iye amaona kuti cikondi cake pa Yehova na Yesu cimakulila - kulila caka na caka . Ndiyeno titakhala kwa nthawi yocepa ku Puerto Rico , tinabwelela ku Ulaya . Monga mmene Baibulo limanenela , “ zonse zimabwelela kufumbi . ” — Mlaliki 3 : 20 . Njila ina imene anthu ofedwa angapezele citonthozo ni kupitila mumpingo wacikhristu . Kugwila naye nchito kunakulitsa cikhumbo canga cokatumikila kudziko lina . ” Kucita zimenezi kungakuthandizeni kudziŵa bwino malamulo a Yehova na mfundo zake . Zoipa zonse zidzatha padziko lapansi , ndipo a khamu lalikulu adzapulumuka mbali yomaliza ya cisautso cacikulu . Kukonzekela kukadzatha , ukwati wa Mwanawankhosa udzayamba . Conco ulosi wa pa Danieli capitala 4 ukukhudza Ufumu wa Mulungu , siconco kodi ? Monga Akristu , timakhulupilila kuti Yesu , “ Mwana wa Mulungu ” * anabwela padziko lapansi n’kukhala Mesiya . Kodi Yesu anaonetsanso bwanji kuti ndi wozindikila ? Mwacionekele , mau ake amphamvu ndi ocititsa mantha anali kumveka mbali zonse m’cigwaco pamene anali kunyoza asilikali a Isiraeli ndi mfumu yawo Sauli . Mwachingilanso nyumba yake ndi ciliconse cimene ali naco . . . Ine ndinati , “ Uli ku China ? ” Akatswili a mbili yakale amati dziko la Roma “ linavekedwa Cikhiristu ” panthawi ya ulamulilo wa Theodosius . 51 : 1 - 17 ) M’malo molola cikumbumtima cacisoni kum’khwethemulilatu , Davide anatengelapo phunzilo pa zolakwa zake . N’cifukwa ciani mtumiki wa Yehova wokhulupilika ayenela kukhala wokondwela , ngakhale pamene zinthu si zili bwino mu umoyo wake ? ANTHU ENA AMAKHULUPILILA KUTI . . . Anali kuona kuti kugonana kunali kudetsa munthu , ndipo sikunali kugwilizana ndi nchito za m’busa . Yehova si woweluza wouma mtima amene amangofuna kulanga atumiki ake . Ine ndi Angie tinakwatilana mu April 1958 , ndipo monga banja , tasangalala ndi mautumiki osiyana - siyana . N’nakondwela kuphunzila Baibo madzulo a tsiku limenelo . Kodi Yobu anali kungofuna zinthu zosatheka ? 8 : 7 ; 11 : 5 . Conco , tiyeni tione mmene njila zimenezi zathandizila Paul , Janet , ndi Alona kulimbana ndi nkhawa . Zitsanzo zimenezi zionetsa bwino kuti anthu a Yehova afunika kugwilitsitsa colungama na kudana ndi coipa . Kodi Yehova anayankha mapemphelo ake ? Zingatheke bwanji kuti Mkristu atengeke ndi khalidwe laciwelewele ? ( b ) Tiphunzilapo ciani pa citsanzo coipa ca Kora , Datani , ndi Abiramu ? Cimathandizanso kuti munthu akhale na mtendele wa m’maganizo na umoyo wacimwemwe . Ndinali kuphunzila Baibulo ndi anthu ambili , ndipo anai anabatizidwa . A Yohane : Iyai , si copepuka . M’fanizo la kapolo wokhulupilika ndi wanzelu , Yesu anachula za kapolo woipa amene anali kuzunza akapolo anzake . Katswili wothandiza anthu kulankhula anatiuza mmene tingakambile naye bwino . Iye anakamba kuti tizinyamula manja m’mwamba tikamufunsa kuti ayankhe inde kapena ai . Kucita izi kudzatilimbikitsa kutsatila malangizo ouzilidwa akuti : “ Ciwalo cimodzi cikalemekezedwa , ziwalo zina zonse zimasangalalila naco limodzi . ” ( 1 Akor . Petulo Khala bata ! ” Tifunika kukhala osamala munthu wina akatipatsa malangizo okhudza thanzi lathu Mwina imwe mukumbukila nthawi ina pamene Mulungu anakuthandizani ndi kukutsogolelani kupitila m’Mau ake . Popemphelela abale athu kwa Yehova , tifunika kuchula mwacindunji mavuto amene akukumana nao . Mutu wa banja afunika kuiganizila mosamala nkhaniyi , kuipemphelela , ndi kufunsako mkazi ndi ana ake . N’zoona kuti Yehova amakhululukila ocimwa amene alapa , koma amafuna kuti tiziyesetsa kulimbana ndi zilakolako zathu za ucimo . PITILIZANIBE KUONETSA KHALIDWE LOPAMBANA MU ULALIKI 20 : 4 . Robert Butler Kodi mwatsimikiza mtima kuti mudzalimbana ndi mayeselo pofuna kupeza madalitso a Yehova ? Munthu amene tifunika kutengela monga citsanzo cathu ni Khristu . 9 : 11 - 15 ) Mipingo ndi anthu ena anali kuwathandiza modzifunila . Ni mmenenso zilili na mavuto a m’banja . Mu 1382 , Baibo ya Cizungu ya Wycliffe inayamba kufalitsidwa . Anthu ambili anganyalanyaze mfundo imeneyi , koma zinthu zapadela zimene zakhala zikucitika kuyambila 1914 ziyenela kutipangitsa kukhulupilila kuti Ufumu wa Mulungu udzacitapo kanthu posacedwapa . M’BADWO UWU SUDZATHA WONSE ( b ) Kodi Mikayeli anaonetsa bwanji kuti ndi wodzicepetsa ? Komabe , nkhani yaikulu kwambili imene ikhudza anthu onse ni kucilikiza ucifumu wa Yehova . 7 : 17 ; 21 : 1 - 4 . Cizoloŵezi cimeneci cimatigwilizanitsa na kutikumbutsa kuti ena adzatithandiza tikakumana na mavuto . ” — Robin . ya May 8 , 2003 , masamba 26 - 29 , ndi yacingelezi ya January 22 , 1995 , masamba 11 - 15 . ( Buku Lopatulika ) * Komanso , makhalidwe amenewa ni mbali ya “ umunthu watsopano . ” Kodi mukanacilikiza nchito yaikulu imeneyo ? Iye anafunsa m’bale Stephen kuti : “ Kodi ‘ nsautso ’ imeneyi n’ciani ? M’nkhani imeneyo muli malangizo ambili othandiza , ndipo muli kabokosi kamene munthu angadule ndi kukasunga kuti azikagwilitsila nchito pa phunzilo laumwini . N’cifukwa ciani gulu la Yehova linamasulila Baibulo la Dziko Latsopano ? Koma kodi ‘ anzathu ’ ndani ? Ngati ndinu mlongo , kodi mungathandize makolo acitsikana kukhalabe olimba mwakuuzimu ngakhale kuti akusamalila ana ? Paul anakambanso kuti : “ Maneba ambili anasiya mabanja ao ndi anzao , n’kupita ku maiko ena kuti akapezeko umoyo wabwino . Tsopano , lekani ndikusimbileni za miting’i imene ndachula kuciyambi kwa nkhani ino . Koma anapelekanso cenjezo lakuti sayenela kumuona monga mdani . ( 2 Ates . 5 : 33 . “ Yehova azidzakutsogolelani nthawi zonse . ” — YES . Kapena mufunika kuulimbitsa ? ▪ Yembekezelanibe ! Jimmy anali kufunsa amai ake kuti , “ Munandisiila ciani ? ” Ni makhalidwe ati olingana ndi a nyama amene anthu ambili ali nawo ? Nanga n’ciani cinathandiza ena kusintha ? N’ciani cidzatithandiza kulimbitsa cikhulupililo cathu cakuti Ufumu wa Mesiya udzakwanilitsa cifunilo ca Mulungu ponena za anthu ? Macaputa na Mavesi , Na . Kulinso ofalitsa pafupifupi 600 amene amatumikila m’mipingo 16 komanso tumagulu 6 ndipo amagwilitsila nchito cinenelo Camanja ca ku Panama Njila ina imene mungalaŵile ubwino wa Yehova ni kuona mmene iye akukuthandizilani pamene muuzako ena za cikhulupililo canu . Conco , n’kutheka kuti analibe kopeza ndalama zogulila zakudya ndi zinthu zina zofunikila anthu okwana 20 kapena kuposelapo . Amanenanso kuti podzafika kumapeto kwa zaka za m’ma 2000 , anthu 1 biliyoni adzafa cifukwa cokoka fodya . Sadzawalila malilo , kuwasonkhanitsa pamodzi , kapena kuwaika m’manda . Ngati mwamukhulukila , kodi ubwenzi wanu ungakhalebe wolimba monga mmene unalili poyamba ? ( b ) Kodi Yehova anadalitsa bwanji Elisa cifukwa cokhala wokhulupilika ? Ŵelengani Agalatiya 2 : 11 - 14 . Koma palinso zina zambili . Zina zimene akatswili amalosela zimacitika , koma zambili sizimacitika . Iye ndi akazi ena anali kuyendela pamodzi ndi Yesu ndiponso atumwi ake . — Luka 8 : 1 - 3 . Rabeka anazindikila kuti mwamunayo wacokela kutali . Kodi dziko lidzashokewa na moto ? Kodi Yehova wapatsa a nkhosa zina mwai wotani ? Iye anati : “ Ndimayamikila kwambili kuti dipo la Yesu landithandiza kukhala paubale wolimba ndi Yehova , Mfumu ya cilengedwe conse . Ndine wokondwa kuti ndimathandiza ena kudziŵa dzina lake laulemelelo . ” ( Luka 17 : 21 ) Usiku wakuti maŵa Yesu aphedwa , iye anapanga “ pangano la ufumu ” ndi otsatila ake . Anthu aononga zinthu zimene zimacilikiza moyo padziko lapansi monga mpweya umene timapuma , nyama , zomela , ndi nyanja . Mmene Yehova amaonela akazi zinaonekela bwino pamene analenga Hava wangwilo . Iye anamulenganso kukhala mthandizi wabwino wa Adamu osati kapolo . M’malomwake , amaona mumtima ndipo amaona mmene aliyense wa ife alili . Patapita nthawi , zinthu zinafika poipa kwambili . Tuakacisi Topatulika Kukalambila ? Zimenezi zinadzutsa funso lonena za ulamulilo lakuti : Ndani woyenelela kulamulila ? Davide anazindikila kuti wacimwila Yehova . — 2 Samueli 12 : 1 - 7 , 13 . Onani kabokosi kakuti “ Kodi Tuakacisi n’Ciani ? ” Cinthu cimene cinali cofunika kwambili kwa iye ndi kuika patsogolo zofuna za Mulungu wake , Yehova , osati zofuna zake . Pankhani ya cikwati masiku ano , Mau a Mulungu amatipatsa malangizo othandiza . Mmene timacitila tikakumana ndi ciyeso zimaonetsa ngati timaona Yehova monga woyenela kulamulila cilengedwe conse kapena ai . Kodi Ella anafunikila kuopa anthu kapena kukhulupilila Yehova ? MBILI YANGA : NDINALI M’GULU LA ZIGAŴENGA Conco , ndi kupanda nzelu kuganiza kuti mtundu wina ndi wapamwamba kuposa wina . Nanga bwanji ponena za Mboni za Yehova ? Daniel , amene ali ndi zaka 25 ndipo amagwila nchito yomangamanga , anati : “ Ndiganiza kuti kugwila nchito mwamphamvu n’kosangalatsa kwambili , makamaka munthu akakhala ndi zolinga zabwino zogwilila nchitoyo . Anakambanso kuti “ malipilo a ucimo ndi imfa . ” Kodi pali makonzedwe otani othandiza kuti Nyumba za Ufumu zatsopano zimangidwe ? Amacita izi m’njila zingapo . N’cifukwa ciani Mkhristu amene wacita chimo lalikulu ayenela kupempha thandizo kwa akulu ? ( Maliko 13 : 32 , 33 ) N’zoonekelatu kuti Mulungu ( “ Atate ” ) waika “ nthawi yoikidwilatu ” pamene mapeto adzafika . Jairo anayankha funso limeneli mwa kukweza maso ake m’mwamba . Inde , cilipo . Cina , tidzayamba kuona anthu a m’gawo lathu ndi maphunzilo athu a Baibulo moyenelela . Aliyense wa ife ayenela kudzifunsa kuti , ‘ Kodi anthu amamasuka kundipempha kuti ndiwathandize akakumana ndi mavuto ? ’ Masiku ano , madokotala ndi anthu ena amalimbikitsa anthu kupeleka magazi n’colinga copulumutsa moyo . Kodi akulu angatithandize bwanji kukhala acangu ndi ogalamuka mwauzimu ? Ngakhale kuti panthawiyo Ophunzila Baibulo sanali kumvetsetsa nkhani ya kusatengako mbali m’nkhondo , zocita zawo zinali kusiyana kwambili ndi za anthu amene anali kucilikiza nkhondo . ( Aheberi 13 : 7 , 17 ) Nthawi zina , kucita zimenezi kumakhala kovuta . Ife tonse tidzakhala ana a Mulungu . — Aroma 8 : 21 . M’bale Mumba : Mwina zimenezo n’zoona . Kodi Mau a Mulungu tingawaseŵenzetse bwanji moyenela mu ulaliki ? 2 , 3 . ( a ) N’ciani cionetsa kuti kusonyeza cifundo ni mbali ya cibadwa ca anthu ? Kuti makolo alandile thandizo lofunika , ana ayenela kuŵaimilako , kuŵathandiza pa mbali zofunikila kulemba ndi kuŵapeleka kulikonse kumene afunika kupita ndi zina zake . — Miy . ( a ) Kodi Yosefe anaonetsa bwanji kudziletsa pocita zinthu na abale ake ? Asanabwele padziko lapansi , Mwana woyamba kubadwa wa Mulungu anati : “ Yehova anandipanga monga ciyambi ca njila yake . . . 139 : 23 , 24 ) Kodi timamupempha nthawi zonse kuti atithandize kukhalabe okhulupilika pamene takumana ndi ciyeso ? — Mat . N’cifukwa Ciani Timalalikila ? Ngakhale n’conco , Toñi anapepesabe kwa mzimayiyo . Tifunika kuzindikila kuti sitingapewe mavuto obwela ndi ukalamba . Conco tingafunse kuti , “ Kodi Yehova amafuna kuti tikhale anthu otani maka - maka ? ” Kusiilana Citsanzo Cabwino ( T . Yehova amatidalitsa ngati tigwilizana pocita cifunilo cake . Zinaonekelatu kuti anthu ambili anali kufuna kumvela uthenga umene n’nali kuwalalikila . N’nababwa mu 1923 mumzinda wa Chatham , Kent , ku England . Cifukwa ku Myanmar kuli ofalitsa uthenga wabwino 4,200 cabe , koma m’dzikolo muli anthu 55 miliyoni . 3 Phunzilani Kukhala Wodziletsa Nthawi ingafike pamene simungathenso kusamalila okalamba panyumba . 43 : 33 ; Deut . ( Yeremiya 10 : 23 ) Ulamulilo wa Mulungu wokha ndi umene udzabweletsa mtendele weniweni ndi cisangalalo . Inuyotu munanena kuti , ‘ Mosakayikila m’pang’ono pomwe ndidzakusamalila , ndipo ndidzaculukitsa mbewu yako ngati mcenga wa kunyanja . ’ ” Kodi atumiki a pa Beteli ndi atumiki a pa Nyumba za Misonkhano amacita utumiki wotani ? Atate anagwilizana ndi zimene Amai anakamba . Komabe , tikukhala m’dziko loipa . Pakuti monga mwa Adamu onse akufa , momwemonso mwa Kristu onse adzapatsidwa moyo . ” — 1 Akorinto 15 : 20 - 22 . Kodi tiphunzilapo ciani pa masomphenya a Ezekieli amenewa ? ( b ) Kodi mumapeza bwanji nthawi yoŵelenga Baibo ? Conco , n’kofunika kwambili kuti wacicepele aganizile mafunso amenewa asanapange cosankha cacikulu cobatizika . ‘ Kodi zovala zanga zimaonetsa kuti ndine wotsatila wa Kristu ? Ni mmenenso Mwiisiraeli wina wolemela dzina lake Boazi anachulila Rute , mkazi wacimoabu . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene makhalidwe a Yesu monga cikondi , kudzicepetsa , ndi kuzindikila angakuthandizileni kuphunzitsa ana anu acinyamata kutumikila Yehova . Anacita izi olo kuti ambili anali kumuzonda . Conco nsembe ya Yesu ndi mphatso imene Mulungu wapeleka kwa inunso . koma zikuoneka kuti iye sanacite zimenezo . ( Onani palagilafu 18 , 19 ) Anatinso , “ pambuyo pake , n’naitanidwa ku Sukulu ya Giliyadi . Koma n’nali kuopa kupita kudziko lacilendo kumene kunalibe anzanga . ” Yehova anamvetsetsa zofooka za Eliya ndipo anatumiza mngelo kukam’thandiza . ( 1 Ates . 5 : 15 ) Mulungu sakondwela ngati tisunga cakukhosi , ndipo kucita zimenezo kungakhale monga kudziyatsila moto umene ungativulaze . Ndithudi , n’zolimbikitsa kwambili kuona acinyamata ambili akusankha kutumikila Yehova . Popeza kuti ndinakulila pa famu , ndinayamba kulakalaka umoyo wosalila zambili wa kumudzi . Mtumwi Petulo ananena kuti Yesu anacita zozizwitsa , kapena kuti “ zodabwitsa . ” Kodi zimene wafotokoza zikumveka zacilendo ? N’zosadabwitsa kuti anthu ambili masiku ano asintha kwambili umoyo wawo cifukwa cophunzila Mau a Mulungu . ( Mat . 24 : 45 - 47 ) Motsogoleledwa ndi mzimu woyela , amafufuza Malemba kuti apeleke malangizo oyenela a mmene gulu lifunika kuyendela pogwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo . Nanga n’cifukwa ciani ? Nanga Mboni za Yehova zinacita bwanji panthawi ya nkhondo ? Tikamapatula nthawi ‘ yosinkha - sinkha ’ malamulo a Mulungu na mfundo zake , timayamba kucita zinthu mwanzelu komanso mozindikila kwambili . Tisalole ciliconse kusokoneza cikondi cathu pa Yehova cimene tinaonetsa poyamba . — Chiv . ( Aroma 12 : 11 ) Kucita zimenezi kumaonetsa kuti mapemphelo athu ni ocokela pansi pa mtima , ndipo Yehova amatidalitsa . 35 : 5 ) Mwiisiraeli aliyense anali ndi ufulu wopeleka copeleka ciliconse caufulu cimene akanakwanitsa mosasamala kanthu za kuculuka kwake malinga ngati copelekaco cinali cakuti angathe kucigwilitsila nchito pomanga malo olambilila . Cotelo anaitanitsa Uriya ndi kumunyengelela kuti apite kunyumba kwake . Kuwonjezela apo , kulephela kukamba na ena m’cinenelo cacilendo kungativutitse maganizo ndi kutifoketsa mwauzimu . Paulo anati : “ Muzitsimikizila kuti zinthu zofunika kwambili ndi ziti . ” Mosakayikila , Akhristu okhulupilika sanafune kufikila kunyumba kwa Diotirefe olo kuti zinali zotheka kutelo . Amadziŵanso pamene munthu ayenela kucitilidwa cifundo kapena ai . Ngati vutolo likupitililabe ndipo ena akuvutikabe ndi fungo la pelefyumu , mungakonze zowajambulila misonkhano kapena kuwalumikiza pafoni kuti azimvetsela misonkhanoyo ali kunyumba , monga mmene zimakhalila ndi anthu ena amene sakwanitsa kuyenda . Molingana ndi anthu amenewa , mukhoza kuona kuti Mulungu amakwanilitsa lonjezo lolimbikitsa ili : “ Mofanana ndi munthu amene mayi ake amamutonthoza , inenso ndidzakutonthozani anthu inu . ” — Yesaya 66 : 13 . Conco , ophunzila a Yesu anafunika kuthetsa cidani na tsankho m’mitima yawo . A Zimba : Kodi n’zotheka kundifotokozela tanthauzo la ulosi wa Danieli ? N’cifukwa ciani anthu okonda ndalama sapeza cimwemwe ? Kodi n’ciani cimene Yesu anacita kuti anthu ayanjanenso ndi Mulungu ? Mwacitsanzo , a m’banja la Beteli ena ku United States anawapatsa mautumiki ena ndi kuwatumiza m’mipingo ndipo adalitsidwa kwambili m’mautumiki ena a nthawi zonse . Kutsatila mfundo za m’Baibulo kumatipindulitsa mwa kuuzimu ndipo kumatithandiza kupeza zosoŵa zakuthupi . — Miy . Yehova anacita zimenezi pamene anali kukhazikitsa mpingo wacikhiristu . Conco anatenga cakudya coculuka n’kupatsa Davide ndi anyamata ake . Yesu analonjeza onse amene anali ovutika ndi olemedwa ndi mavuto ao kuti : “ Bwelani kwa ine , . . . ndipo ndidzakutsitsimutsani . ” Popeza anali atagona , Yaeli analimba mtima n’kumupha . ( Ower . Adamu anafunika kusankha kumvela Mlengi wake kapena Hava . Ngakhale kuti n’cosavuta kuyamba khalidwe limeneli , sizitanthauza kuti n’labwino . ” 13 : 4 . ( a ) N’cifukwa ciani malangizo amene abale anapeleka okhudza kuphunzitsa ena ndi ocititsa cidwi ? Timayesetsanso kulalikila anthu m’malo okwelela mabasi , m’masitesheni a sitima , m’malo oimikapo magalimoto , kuphatikizapo , m’miseu , ndi m’misika . Kodi fuko la “ Efuraimu ” linali kuimila ciani ? A Zulu : Ndikutanthauza kuti pamene mafumu aciisiraeli anali kulamulila m’Yelusalemu m’nthawi za Baibulo , zinali ngati akukhala pa “ mpando wacifumu wa Yehova . ” ( Maliko 10 : 29 , 30 ) Ngati mumasonkhana nthawi zonse , mukhoza kukhala tate , mai , m’bale , kapena mlongo wa Mkristu wina mumpingo wanu . 13 : 19 - 22 ; Maliko 4 : 19 ) Kukamba zoona , ngati sitisamala , nkhawa za moyo zingatisoceletse ndi kutifooketsa mwauzimu . M’busa wabwino amagwilitsila nchito ndodo potsogolela ndi poteteza nkhosa zake . Ndipo kaonedwe kanga ka zinthu mu umoyo kanasinthilatu . Conco , n’zacidziŵikile kuti nkhani ya ukapolo na ufulu inali mkamwa - mkamwa pakati pa anthu wamba , kuphatikizapo Akhristu . Tchelani khutu kwa ine kuti mudye zabwino , ndiponso kuti moyo wanu usangalale kwambili ndi zakudya zamafuta . ” — Yes . Koma pamene anakhala mboni analekelatu kuvina ngakhale pa maphwando a Mboni , poopela kuti anagayambenso kuganizila zakale . Cifukwa cokhala ndi khalidwe la kufatsa , ambili amene kale anali aukali lelo ni acimwemwe . ( Mateyu 11 : 4 , 5 ) Mosiyana ndi atsogoleli a zipembedzo , Yesu anali kuphunzitsa anthu amene anali kufuna kudziŵa za Mulungu . Mwacitsanso , kukhala na zolinga zapamwamba zakuthupi , kaduka , ndi kusalamulila mkwiyo , zapangitsa ambili kukhala odzikweza . Tsiku lotsatila , anayamba kudzitama cifukwa ca kupha munthu . Zimene n’naona pa msonkhanowo zinapangitsa kuti niyambe kuphunzila Baibo na Mboni , na kupezeka pa misonkhano yawo ya mpingo . Mofananamo , sitiyenela kutalikilana ndi abale athu mwa kuphonya misonkhano . Nsangala zimathandiza . Mwina iye anacita izi pofuna kupewa mavuto amene analoseledwa kuti adzacitikila mbadwa za Abulahamu . M’mafanizo onse aŵili , mbuye amaimila Yesu . Akapolo amaimila ophunzila ake odzozedwa . “ Sandulikani mwa kusintha maganizo anu . ” — AROMA 12 : 2 . 24 : 21 , 22 ) Sitidziŵa bwino - bwino zimene zidzacitikila aliyense wa ife . Ndipo ngati mumavutika maganizo cifukwa cakuti wacibale wanu ndi wocotsedwa , muuzeni Yehova nkhawa yanu m’pemphelo . Anali kudziŵa kuti Isaki sanali cabe mwana wamba , koma anali na mbali yofunika kwambili pa colinga ca Yehova . Ngati mulibe colinga cocita upainiya pakali pano , kodi muyenela kucita ciani ? Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Adzakutengelani kwa abwanamkubwa ndi mafumu cifukwa ca ine , kuti ukhale umboni kwa iwo ndi kwa anthu a mitundu ina . ” ( Mat . Conco , tiyenela kutengela citsanzo ca Yesu mwa kumvela ena cifundo . — 1 Pet . Yesu anatiphunzitsa mfundo yofunika kwambili imeneyi paumoyo . Buku la Genesis limakamba cabe kuti : “ Inoki anayendabe ndi Mulungu woona . Panthawiyo , Yerusalemu , amene anali kuwapangitsa kukondwela kwambili mwa Yehova , anali atawonongedwa . ( Sal . Kodi ndani adzathetsa mavuto a anthu ? M’Baibo muli malemba ambili oonetsa kuti m’nthawi ya atumwi , ophunzila atsopano a Khristu anali kudziŵa bwino kufunika kwa ubatizo . Khalidwe limeneli linayambila mu m’badwo waciŵili , pamene Kaini anapha m’bale wake Abele . Zaka zambili m’mbuyomo , wamasalimo anakamba kuti tifunika kuyang’ana kwa Yehova pamene tifuna thandizo . Tingapitilize kugwila nchitoyi ngati tipanga zosankha zimene sizingadodometse utumiki wathu . Tingamuuze Mlengi mavuto athu amene tili nao . Ndipo ngati timacelezana , kupatsana zinthu mowoloŵa manja , kukhululukilana , ndi kukomelana mtima , Yehova amaonanso zimenezo . — Aheb . Yesetsani kuzindikila mbali imene mumalephela kudziletsa . Patapita miyezi inai , ndinaikidwa kukhala mpainiya wapadela ndi mtumiki wa mpingo mu mpingo waung’ono m’cigawo ca Carinthia , m’tauni ya Spittal an der Drau . Komabe , kusamalila munthu wodwala n’kovuta . 4 : 8 ; Miy . Ndipo ponena za vinyo iye anati : “ Vinyoyu akuimila ‘ magazi anga a pangano , ’ amene adzakhetsedwa cifukwa ca anthu ambili . ” N’cifukwa ciani anthu a ku Poland anasamukila ku France ? Masiku ano anthu ambili akuvutika cifukwa ndi osauka kwambili pamene ena ndi olemela kwambili . Kodi timakhulupililadi kuti Yehova adzatipatsa zinthu zimene timafunikila ? ( 1 Yoh . 1 : 9 ) Tifunikanso kufikila akulu , kuti atipatse cithandizo cauzimu . Pokamba za anthu ambili amene anaphedwa , Baibo imati : “ [ Mfumu Nebukadinezara ] inapha anyamata awo ndi lupanga m’nyumba yopatulika . Sinacitile cisoni mnyamata kapena namwali , wacikulile kapena nkhalamba yothelatu . . . . Asaduki , amene sanali kukhulupilila ciukililo , pofuna kutapa m’kamwa Yesu anam’funsa za ciukililo ndi za cikwati ca pacilamu . Mwacitsanzo , masiku ano acicepele ku sukulu amatunthiwa kuti alimbikile kwambili maphunzilo awo kuti akakhale na mwayi wophunzila ku mayunivesiti apamwamba . 5 : 13 ) Cimene cionetsa zimenezi n’cakuti mngeloyo anavininkhila ciwiyaco mwamsanga . Pali zambili zimene tifunika kucita . ( Luka 20 : 37 , 38 ) Pa nthawi ino , tili na zifukwa zomveka zokhalila na cikhulupililo ngati ca Paulo , amene anati : “ Ndili ndi ciyembekezo mwa Mulungu , . . . kuti kudzakhala kuuka . ” — Mac . Kupeza nthawi yoceza na banja locokela ku dziko lina , kudzatipatsa mpata wabwino wowayamikila pa kuyesetsa kuti agwilizane ndi cikhalidwe cathu . Pangano la Davide limatitsimikizila ciani ponena za ulamulilo wa Mesiya ? Mwacionekele , mungafune kumvetsela zoonjezeleka . Tsopano nili na mtendele m’maganizo . ” Mkulu wina wa ku France dzina lake Jean - Claude anati : “ Ndikamaphunzitsa wophunzila , colinga canga cimakhala kumuthandiza kukonda zinthu zakuuzimu . Mwacitsanso , ganizilani citsanzo ca Yesu . Iye akuti : “ Ndazindikila kuti Yehova amatilimbikitsa pa mavuto ndi kuti tili ndi zinthu zabwino zambili kuposa mavuto . ” Enanso angakhale acibululu , maneba , ndiponso anzathu a kunchito kapena akusukulu amene salambila Yehova . Iwo amaganiza kuti Mulungu afuna kuti tizicita naye mantha . Nkhani yaciŵili ifotokoza kufunika kwa cikhulupililo . Patokha , tikanasoŵa cocita . Komabe patsiku laciŵili , n’nakondwela kwambili kudziŵa kuti pamsonkhanowo panali kagulu ka cinenelo camanja ndipo panalinso womasulila . Apa m’pamene n’nayamba kusangalala na pulogilamu yamsonkhanowo . Ndiponso , pa alaliki a Ufumu a nthawi zonse oposa 1 miliyoni padziko lonse ambili ndi akazi . Mwacitsanzo , m’masiku a Mfumu Hezekiya , Senakeribu , mfumu ya Asuri inaukila Yuda ndi kulanda mizinda yonse yokhala na mipanda yolimba kwambili , kupatulapo Yerusalemu . ( 2 Maf . Baibo imati : “ Yehova anamukwiyila kwambili Solomo cifukwa mtima wake unapatuka kwa Yehova . . . , amene anamuonekela kaŵili konse . Koma Yehova sanacite zinthu mopupuluma pankhaniyi . ( 1 Mafumu 21 : 27 ) Kodi Ahabu anali kusonyeza kulapa ? Ubwenzi umalimba ngati anthu amakambilana momasuka . Onani nkhani yakuti “ Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga ” mu Nsanja ya Olonda ya June 15 , 2004 , masamba 29 - 31 . ANTHU AMENE ANAPINDULA NDI CILUNGAMO CENICENI N’tapeza mayankho pa mafunso anga , n’nadabwa kwambili . Mulimonse mmene zingakhalile , dziŵani kuti Yehova adzakondwela poona khama lanu lofuna kuyanjananso na m’bale wanu , amenenso ni bwenzi lake . Satana amafuna kuti ‘ tidzikomele mtima ’ mwa kudzifunila umoyo wa wofuwofu m’dzikoli n’colinga cakuti tigone mwa kuuzimu . Kodi cikondi na kukoma mtima zingatiteteze bwanji kuti tisakamaniwe mphoto ? N’ciani cinam’thandiza kusamalila udindo waukulu umenewo ? Komabe , makambilano amenewa safunika kucitokakamiza . M’malomwake , azicitika momasuka pamene mukuceza nthawi iliyonse . Anthu ambili anali kulankhula Cigiliki , ndipo zimenezi zinathandiza kuti mipingo izicita zinthu mogwilizana . Lonjezo limeneli ndi nkhani yaikulu kwambili . Kodi zimenezi zinam’khudza bwanji Timoteyo ? Koma zimene zinacitikila Ribeiro wa ku Brazil , zionetsa kuti n’zotheka kuthetsa cizoloŵezi cimeneci . 10 : 11 - 13 ; Chiv . 14 : 6 ) Robert , amene watumikila monga mpainiya kwa zaka zoposa 30 , anati : “ Kuseŵenzela pamodzi na angelo amene amadziŵa bwino zocitika mu umoyo wa anthu n’kokondweletsa . ” ( b ) Kodi mwatsimikiza mtima kucita ciani ? ( Yes . 45 : 18 ) Masiku ano , anthu angasankhe kusakwatila kapena kukwatila koma osabeleka ana . Ndipo kucita izi si kosemphana na cifunilo ca Yehova . Nanga kodi m’Baibo muli mfundo iliyonse imene ingatithandize kudziŵa nthawi pamene akufa adzauka ? Yesu anaonetsa kuti mkazi wamasiye ndiponso copeleka cake zinali zamtengo wapatali kwa Yehova . Paulo anauzilidwa kulemba kuti : “ Ine , . . . ndikukucondelelani kuti muziyenda moyenela kuitana kumene munaitanidwa nako . Muziyenda modzicepetsa nthawi zonse , mofatsa , moleza mtima , ndiponso mololelana m’cikondi . Muziyesetsa ndi mtima wonse kusunga umodzi wathu mwa mzimuwo , ndi mwamtendele monga comangila cotigwilizanitsa . ” ( Aef . Yehova akutithandiza kuti ‘ tizimutumikila mogwilizana . ’ Nafenso tisamaone cabe maonekedwe akunja , koma tizionetsa cikondi ceni - ceni , ndi kukhala oleza mtima na anthu amitundu yonse . ( 1 Tim . ( Yohane 11 : 21 - 27 ) Ngakhale n’conco , Marita anali wopanda ungwilo . Tifunika kukhala acifundo . Mukalemba mfundo zofunika pa nkhani ya onse , pamisonkhano yapadela ndi yacigawo , muzipeza nthawi yobwelelamo . ( Agal . 6 : 5 ) Muriel , amene tamuchula kuciyambi kwa nkhani ino , anavomeleza kuti analolela kucita zimene mwana wawo anali kufuna n’colinga cakuti iye apindule mwauzimu . Muzikhala na mabwenzi olimbikitsa ndi okoma mtima , koma amenenso angakuuzeni mosapita m’mbali mukalakwitsa zinthu . — Miyambo 13 : 20 ( Machitidwe 2 : 38 ) Komanso , si Akristu onse amene amadzozedwa panthawi imene akubatizidwa . Kenako , anamupangila tiyi ndi kuyamba kuceza naye . Timalimbikitsidwa kuganizila ena makamaka pa misonkhano yacigawo , cifukwa cakuti n’zosatheka kukhala ndi malo apadela a anthu amene amadwala cifukwa ca fungo la pelefyumu . Anthu a Yehova “ Aleke Kucita Zosalungama , ” 7 / 15 Conco ulamulilo wa mafumuwo unali kuimila ulamulilo wa Mulungu . N’zoonekelatu kuti iye ndi woolowa manja , ndipo amatikonda kwambili . — 1 Timoteyo 6 : 17 ; Salimo 145 : 16 . Ndipo ngati tiyesetsa kulola malamulo a Mulungu na mfundo zake kuphunzitsa cikumbumtima cathu , tikhoza kufika “ pa msinkhu waucikulile umene Khristu anafikapo . ” — Aef . Cacikondi : Kulanga koyenela kumazikidwa pa cikondi , osati pa mkwiyo . Akristu odzozedwa adzakhala mafumu pamodzi ndi Yesu kumwamba . ( Aroma 16 : 1 , 12 ) Kodi sitiyamikila kukhala ndi Akristu amenewo m’mipingo yathu ? Anthu atayamba kusamukila m’madela osiyana - siyana padziko lapansi , iwo anasunga nkhani zokhudza munda weni - weni wa Edeni . Nkhani yotsatila idzayankha mafunso amenewa . Koposa zonse , tingapindule ngati titengela cikondi ca Mulungu na kukhululukila ena na mtima wonse . — Akolose 3 : 13 . 5 : 11 - 13 ) Ndipo ngati sanalape , amakhala oipa kwambili monga mmene Petulo anafotokozela . — Ŵelengani 2 Petulo 2 : 20 - 22 . Ngakhale n’conco , ciliconse cimene timacita pothandiza ena kupeza njila ya ku moyo na kupitiliza kuyendamo , cidzathandiza ise pamodzi ndi anthuwo kudzapeza cuma cosatha . — Mat . Pambuyo pa kumva mayankho ao , wansembeyo anati , “ Onse ndi opusa , anapeleka yankho lofanana lakuti ‘ Tikulalikila Uthenga wabwino wa Ufumu . ’ ” Abale okhulupilika anakana kuloŵa usilikali , koma abale 9 pa gulu limenelo anavomela ndipo analandila zovala za usilikali . Kumbukilani mfundo yosatsutsika imene munthu wina , dzina lake Noam Chomsky , analemba . Iye anati : “ Palibe munthu adzacita kuika coonadi m’maganizo mwanu . Satana Amafuna Kutikopa ( Onani palagilafu 12 , 13 ) khalidwe la ciwelewele , kunyada , na zamizimu Anafunikanso kuyembekezela kwa zaka zina 60 kuti adzukulu ake , Esau na Yakobo , abadwe mu 1858 B.C.E . — Aheb . 9 : 26 ) Monga mmene wankhonya amachingila kuti adziteteze kwa mdani wake , nafenso tifunika kudziteteza kwa adani athu . Kodi ndi zinthu ziti zimene mabanja angakambitsilane ? ( Onani mau a munsi . ) ( b ) Tingafotokoze motani zifukwa zimene takanila kupita ku cikwati cimene cidzacitikila m’chalichi ? Zimenezi n’zimene zinacitika m’banja la mneneli wina dzina lake Samueli amene anali ndi mbili yabwino , ndipo anayamba kutumikila Yehova ali mwana kwambili . ( 1 Sam . ( Yobu 1 : 13 - 21 ) Kenako , kunabwela anzake atatu amene anali kunamizila kuti abwela kudzam’tonthoza . ( Aroma 3 : 23 ) Pomveketsa bwino mfundo imeneyi Baibo imati : “ Pitilizani kulolelana ndi kukhululukilana ndi mtima wonse , ngati wina ali ndi cifukwa codandaulila za mnzake . ” — Akolose 3 : 13 . ICI NI CIYEMBEKEZO CABWINO MANINGI ! Moleza mtima fufuzani malangizo amene angakuthandizeni ndi kupeza mayankho a m’Baibulo pa mafunso anu . N’nakumana na Mboni za Yehova koyamba pamene n’nali kukhala m’nyumba za boma zokhala azimayi wosakwatiwa ndi ana awo akhanda . Akulu ndi ofunitsitsa kugwila nchito ya Yehova , ndipo zimenezi zimaonekela ndi mmene amatsogolela mpingo . ( 2 Akor . Koma m’maiko ena , mavuto a zacuma amacititsa acicepele kuona kuti afunika kuthandizila makolo awo kupeza zofunika pa banja . Koma ukawalongoza mfundo inayake m’Baibo , amamvetsela mwachelu . ” Mapangano 6 amene adzakwanilitsa cifunilo ca Mulungu ndi awa : Anthu ambili akaona anthu ena akuvutika na masoka , amafuna kuwaonetsa cifundo . N’cifukwa ninji mufunika kukhala wokhulupilika , woleza mtima , ndi wodalila pemphelo ? Masiku ano otsiliza , kukhala oona mtima kungakhale kovuta cifukwa anthu ambili ni “ odzikonda , ” ndiponso “ okonda ndalama . ” Kuti tisataye cimwemwe cathu , tiyenela kuika maganizo athu pa zabwino zimene tili nazo pa nthawi ino , na kuyembekezela moleza mtima madalitso am’tsogolo . Kodi Malemba monga 1 Yohane 3 : 17 , angatithandize bwanji kukhala acifundo ? Ndipo tikhulupilila kuti n’zotheka kuloŵa mu mpumulo wa Mulungu umenewu . Tayamba kale kucita zoyenela kuti tiloŵemo . Mofananamo , abale ndi alongo anu sadzaiŵala cikondi cimene muli naco pa Mulungu . 8 : 1 - 4 . Kodi ‘ mudzadzipeleka kwa Mulungu monga anthu amene wouka kwa akufa ? ’ 11 : 12 , 13 ) Iye ‘ safulumila kukwiya . ’ Sara ayenela kuti anakulila ku Uri . M’nkhani imeneyi , iye sanakambe mau ozama kapena osafunika kwenikweni pofuna kugometsa anthu . Tiyeni tikambilane mayankho ake . Nkhani yaciŵili ifotokoza mmene atumiki a Yehova amaonetsela kuti amakonda anzao . Aka kanali kaciŵili kuuzidwa kuti ndikhale msilikali wa gulu la nkhondo la dziko la United States . Koma Paulo sanasinthe maganizo . TSAMBA 22 • NYIMBO : 107 , 29 N’ciani cimene tifunika kucita kuti tikapeze ufulu weni - weni ? Kodi utumiki wa pa Beteli umathandiza bwanji acicepele kukhala osangalala ? Yesu anali wokoma mtima , wodzicepetsa ndi wocezeka . Mwa ici , cikhulupililo cathu cinalimba ngako . Cinanso , makonzedwe amenewa amatiphunzitsa kuti iye akatikhululukila , amaiŵalako za chimo limene tinacita . Mame amatsitsimula . Ndipo pa mpikisanowu , tikulimbana ndi adani amene afuna kuticenjeneka , kutigwetsa , kutigonjetsa , ndi kutilanda cimwemwe na mphoto ya mtsogolo . Koma Yesu analonjeza kuti adzawapatsa banja lina limene lidzawakonda ndi kuwasamalila . Conco , tiyeni tiziwakonda abale athu monga mmene Yehova watilamulila . — 1 Yoh . 4 : 20 , 21 . Coyamba , musalole ciliconse , kaya zitsanzo , mafanizo , kapena kakambidwe kanu , kuphimba mfundo ya Malemba amene mwaŵelenga . Zotsatilapo zake n’zakuti , tidzayamba kupanga zosankha zom’kondweletsa , ndipo iye adzatidalitsa . Iwo sanamvele ndi mitima iŵili , koma anaonetsa kuti anali kumbali ya Yehova ndipo anakanilatu kucita zosalungama . Winanso anati : “ Tsopano udindo wanga wotumikila abale ndimauona kukhala wofunika kwambili . ” Kusokonezeka . ( Mat . 25 : 10 ) Mu Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 , tinaphunzila kuti mu ulosi wopezeka pa Mateyu caputala 24 ndi 25 , Yesu anachula za ‘ kubwela ’ kapena kufika kwake nthawi zokwanila 8 . Sitiyenela kuleka kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova ( Onani ndime 16 ndi 17 ) Masiku ano , tonse tingakopeke mosavuta na maganizo a anthu a m’dzikoli cifukwa amafalitsidwa pa ma TV , pa Intaneti , ku nchito , kapena kusukulu . KODI ndinu wacinyamata mumpingo ? Paulo anati : “ Kale ndinali wonyoza Mulungu , wozunza anthu ake ndiponso wacipongwe . 11 : 23 - 26 . Malinga n’zimene Malemba amakamba , tidziŵa kuti masiku ano , Mulungu sangatalikitse moyo wathu kapena kuticilitsa mozizwitsa . Amadziŵa kuti kutumikila Mulungu kumafuna kuti akhale umoyo wosalila zambili m’dziko lino la Satana , ndipo ndi ofunitsitsa kucita zimenezi . Mikhail anakamba kuti : “ Panthawi ina tinapita kukalalikila m’dela limene Mboni zikalibe kulalikilamo , tinapeza mwamuna wina wacikulile amene anatifunsa kuti , ‘ Kodi ndinu alaliki ? ’ N’cifukwa Ciani Anthu Amafa ? Kucokela zaka za m’ma 1500 mpaka m’ma 1800 , kutenga anthu ukapolo kuwacotsa mu Africa ndi kuyenda nawo ku America , anali amodzi mwa malonda opindulitsa kwambili padziko . “ Tsopano amai anga afuna kuti ndiwatumizile mwana wanga kuti akamulele monga mmene io ananditumizila kwa ambuye , koma ndinakana m’njila yakuti asakhumudwe . Ndimayesetsa kukumbukila cikondi canga ca poyamba kwa Yehova , makamaka ndikakumana ndi ziyeso kapena mavuto ena M’nthawi za m’Baibulo , alimi anali kupuntha tiligu pamtetete kuti mphepo iziulutsa mankhusu . Tinathandizanso kulimbitsa kagulu kocepa ka ofalitsa a m’tauni ya Kurganinsk , imene inali pafupi na mzinda wa Armavir . Iye anadziŵa kuti dziko limenelo ndiwo malo abwino amene anafunika kukhalamo , ndiponso kuti mtsogolo kudzakhala kwawo kweni - kweni . Pamene tiuza anthu acidwi za mawebusaiti athu ovomelezeka , timawathandiza kuti azilandila cakudya cauzimu kucokela ku gwelo lokha loyenelela , limene ni “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” Ndipo ngati tiuza ena mmene tapindulila pocita phunzilo laumwini , tingawalimbikitse kuti nawonso aziphunzila Baibulo mwakhama kuti apindule . Akhozanso kunola luso lao lolalikila ndi kukhala ofunitsitsa kucita zambili mu utumiki wa Mulungu . Sitikaikila kuti Yehova ali ndi mphamvu yocilitsa odwala . 35 : 25 ) Koma panali poyenela kwa iye kupilila zimenezi . 22 : 16 - 18 . Poonetsa kusiyana kwa Timoteyo na abale ena , Paulo analemba kuti : “ Ena onse akungofuna za iwo eni , osati za Khristu Yesu . ” ( Afil . 2 : 5 - 10 ) Palibe nthawi yoikika imene iyenela kupitapo kuti munthu abwezedwe mu mpingo . Ngakhale n’conco , ciwembu ca mtundu umenewu , cimene sicicitika - citika pakati pa anthu a Mulungu , sitingacilekelele . Komabe , ena amakamba kuti kuyatsa moto kunali kovuta m’nthawi zakale . Komabe , Yesu anali wokongola mwapadela cifukwa cakuti anali wokhulupilika kwa Yehova ndiponso anali ndi mtima wosagawanika . Tinapitiliza kucita utumiki umenewo mpaka mu 1975 , pamene dziko la Mozambique linakhala ndi ufulu wodzilamulila kucokela ku dziko la Portugal . N’cosankha citi cimene mayi wina anafunika kupanga mwana wake atabadwa ? Nanga n’ciani cinamuthandiza kusankha mwanzelu ? Cinali cifukwa cakuti Petulo ndi ophunzila ena anali otsimikiza kuti Yesu anali moyo , ndi kuti anali kutsogolela nchito imene Mulungu anafuna kuti icitike . Ndinali kuona kuti anali kuphunzila zinthu zabodza monga Felisa . Pamene nkhondo inali kutha , n’naona kuti boma na cipembedzo zinalephela kutithandiza . Patapita nthawi , atate analekadi kuwaletsa , ndipo amai anali kupita ku misonkhano momasuka . Zeynep Cifukwa cakuti anthu ambili anali acidwi kumeneko , M’bale Russell anayendelanso dziko la Ireland paulendo wake wacitatu wopita ku Ulaya . Ngati zimene mumaphunzila mumazikhulupilila na mtima wonse ndipo mwakonzekela bwino , mudzakhala wofunitsitsa kucitila umboni za dzina la Yehova . — Yer . ( Malaki 3 : 10 ) Nanga bwanji za mwana wa Yefita ? Kodi mudzavomela ciitano cimeneci ndi kulola Mulungu kukutetezani m’masiku ovuta ano ? Makolo ena ku America ndi ana awo , amayamikila Yehova akacita cidwi ndi cilengedwe , kapena pamene asangalala ndi zakudya zinazake . * Inde , n’zocititsa cidwi kuona kuti pa anthu 4 alionse m’matauni amenewa , mmodzi ni Mboni ya Yehova . Koma mukaleka kutumikila Yehova cifukwa cokhumudwa , posakhalitsa mudzadzionela mwekha kuti palibe wina aliyense amene amakukondani zeni - zeni , mofanana na makolo anu acikhristu kapena abale na alongo mu mpingo . Nthawi zambili amayamikila tikapita kukaphunzila nawo . Pambuyo pakuti mkulu wakonzekeletsa mtima wa wophunzila , ayenela kumupatsa malangizo oyenelela . Ndipo anamukomela mtima n’kumupatsa dzina loposa lina lililonse . ” — Afil . ( c ) Fotokozani mmene inu panokha mwapindulila cifukwa coŵelenga Mau a Mulungu ndi kuwasinkha - sinkha . Mofananamo , ngati nthawi zonse timadandaula za abale amene Yehova akugwilitsila nchito kutsogolela anthu ake masiku ano , zimaonetsa kuti cikhulupililo cathu mwa Mulungu cayamba kufooka . A Zulu : Kumbukilani kuti mtengo wa mu ulosiwu unali kuimila Mfumu Nebukadinezara . Koposa zonse , Baibo imatiphunzitsa kuti tikhoza kukhala na umoyo waphindu mwa kulambila Mulungu woona , Yehova . Kodi tingathandize bwanji kuyeletsa dzina la Mulungu ? Kumiko anati : “ Anayesa kunilimbikitsa kuti tipite , koma ine n’nali kukana . ( Salimo 119 : 108 ; 2 Akorinto 9 : 7 ) Tikapemphelela zinthu zimenezi ndi kuzisinkhasinkha , tidzapanga cosankha mwanzelu , ndipo Yehova adzatidalitsa . Izi zitanthauza kuti tifunika kupewelatu ciliconse cimene cingatigwetsele m’chimo limeneli , monga kuonelela zamalisece . ( Sal . 119 : 37 ; Mat . Mwa ici , ubwenzi wawo unakhalanso wolimba . Kodi Yobu anaonetsa bwanji kuti anali kum’dziŵa bwino Yehova ? Ngati tiona kuti cithandizo ca mankhwala n’cofunika kwambili kwa ife , ndiye kuti tikuganizila zofuna zathu zokha . ( Gen . 3 : 4 , 5 ) Hava anakhulupilila ndipo anacita zinthu payekha mwa kudya cipatsoco . Mwacitsanzo , pamene Yesu anauza ophunzila ake kuti iye adzaphedwa , Petulo anamuuza kuti adzikomele mtima . Musakhutile ndi duŵa limodzi cabe la coonadi . . . . Kuonjezela apo , mmodzi pa anthu atatu alionse amadwala matenda obwela cifukwa ca kupeleŵela kwa cakudya m’thupi . ” Imatikumbutsanso za kukhulupilika kwa anthu ambili a “ nkhosa zina . ” Zaconco zinali kucitika . * — Dan . Mayankho a mafunso amenewa adzakuthandizani kuona ngati mufuna kubatizidwa mwa kufuna kwanu . Mngelo analamula mlaliki Filipo kupita ku msewu wa kucipululu , wocokela ku Yerusalemu kupita ku Gaza kuti akalalikile Mwiitiyopiya , amene anali kucokela ku Yerusalemu kukalambila . — Machitidwe 8 : 26 - 33 . ( Mateyu 27 : 46 ; Maliko 5 : 41 ; 7 : 34 ; 14 : 36 ) Koma Yehova anaonetsetsa kuti uthenga wa Yesu walembedwa ndi kumasulidwa m’Cigiriki , ndipo m’kupita kwa nthawi unamasulidwanso m’zinenelo zina . Kuwonjezela pamenepo , nimasangalala ndi mgwilizano umene uli pakati pa anthu a Yehova . Kodi makonzedwe amenewa anathandiza bwanji Mboni za Yehova ? Amosi anakamba kuti iye anali m’busa wa nkhosa ndi woboola nkhuyu . Baibulo limati : “ Monga mwa Adamu onse akufa , momwemonso mwa Kristu onse adzapatsidwa moyo . ( Salimo 28 : 7 ) Ndipo coonadi camtengo wapatali cimeneci nidzacisunga kwa moyo wanga wonse . Pewani kudzidalila . Koma sindinaleke kukoka , ndinaona monga n’zosatheka . ” Akristu acipolishi amenewa anali akhama polalikila monga mmene anali kucitila khama panchito ya ku migodi . Kapena kodi mungafune zina zake ? Khalani ndi maganizo oyenela ndipo kumbukilani kuti ena m’banja angakhale ndi maganizo osiyana ndi anu . Mulungu ndi Mwana Wake , Yesu , amakonda anthu amene ndi oona mtima ndi opanda cinyengo . A Zimba : N’zoona , cifukwa cakuti ndinaŵelenga cofalitsa canu cimene cinakamba kuti Ufumu wa Mulungu unayamba kulamulila mu 1914 . ( Yobu 22 : 1 - 3 ) Kodi mungayankhe bwanji mafunso amenewa ? Kulandila cipepeso na kukhululuka kumafuna kudzicepetsa kwambili . ” — Kimberly . Ngati mufuna kuti anthu azikudalilani kwambili kapena ngati mufuna kuti anthu amene amakukayikilani ayambenso kukudalilani , mungacite zotsatilazi . Zitatelo , Datani ndi Abiramu anatuluka n’kuima pamakomo a mahema ao , limodzi ndi akazi ao , ana ao . ” Tiyeni tione umboni wake . Ku Quetta , n’nakumana na m’bale George Singh , amene anali mpainiya wapadela wa zaka za m’ma 20 . Mlengalenga . Lofalitsidwa m’caka ca 1995 koma tsopano silisindikizidwanso . Koma Satana anali kufuna kuti iye acite zimenezo . Ngakhale kuti nthawi zina Petulo analephela kugonjetsa mtima wodzikonda , citsanzo cake cimatilimbikitsa . Tingacite ciani kuti tithetse manyazi n’kumaimba momasuka nyimbo zotamanda Yehova ? N’cifukwa ciani kuyamikila cisomo ca Mulungu kumatilimbikitsa kupewa macimo alionse ? TSAMBA 3 • NYIMBO : 123 , 121 5 : 13 - 15 ; 6 : 2 , 21 ) Panthawi ina , Mfumu Hezekiya anakumana ndi gulu la asilikali a Asuri amphamvu amene anaopseza kuti adzawononga Yerusalemu . N’cifukwa cakuti anatilenga kuti tizicita zinthu zakuuzimu ndi kuonetsa cikondi . ( 1 Akorinto 6 : 9 , 10 ) Komabe , tikali opanda ungwilo . Lomba tiyeni tikambilane fanizo limenelo . Tizikumbukila zimenezi nthawi zonse pamene tilalikila . ( 1 Timoteyo 1 : 5 ) Ngati timaphunzitsa bwino cikumbumtima cathu ndi kucitsatila , timakonda kwambili Yehova ndipo cikhulupililo cathu cimalimba . Kumbukilani kuti pamene Yesu anayelekezela masiku athu ano na masiku a Nowa , sanagogomeze za khalidwe la ciwawa kapena la ciwelewele , koma za kuopsa konyalanyaza zinthu zauzimu . — Ŵelengani Mateyu 24 : 36 - 39 . Izi zimapangitsa anthu ena kuwakhalilako patali . Izi n’zofanana ndi mmene mwana amatengela zocita za makolo ake . ( Agal . 5 : 22 , 23 ) Kuti timveketse bwino tanthauzo la mau akuti “ munthu wokonda zinthu zauzimu , ” ganizilani citsanzo ici : Ngati munthu amadziŵa kwambili zamalonda , tingakambe kuti ni wokonda bizinesi . Monga mmene ofufuza golide amacitila kuti apeze golide , muyenela kuti inunso munacita khama kuti mupeze cuma cakuuzimu . “ Koma ngati munthu akukonda Mulungu , ameneyo amadziŵika kwa Mulungu . ” — 1 AKOR . Kukhala wodzicepetsa kumatanthauza kupewa kudzikuza kapena kunyada . Anthu amene amapita mumseu umenewu amaona cizindikilo ca JW.ORG cimene cakhalapo kucokela pamene anayamba kumanga Kugona nthawi yaitali . Panthawi imeneyo , Mulungu anavomeleza mwambo umenewu pakati pa anthu ake . Koma Yesu atabwela anaika lamulo lakuti anthu asakwatile mitala . ( Mateyu 19 : 4 - 6 ) Yakobo anali ndi ana 14 amene sanali a mimba imodzi . 5 : 15 ; 13 : 5 ) Mwina mungamufunse kuti : ‘ Kodi munamulonjeza ciani Mulungu pamene munadzipeleka kwa iye ? ’ Kapena ndani amene angatiuze zinthu zimene zidzayambilile kucitika ? N’cifukwa ciani zimenezi n’zocititsa cidwi ? Kodi Yehova anam’dalitsa bwanji Mariya ? NYIMBO : 18 , 91 Koma kodi tingaleke bwanji kucita zosalungama ? YEHOVA MULUNGU anapatsa anthu cinenelo monga mphatso . Yesaya anapatsidwa nchito imeneyi m’caka cothela ca ulamulilo wa Mfumu Uziya , kapena kuti mu 778 B.C.E . Ndithudi , ndife okondwa kuti Yehova anakonza zakuti pakhale nchito yoyenga mwa kuuzimu kuti ayeletse anthu apadela kuti acite nchito zabwino . * Popeza kuti mukucita zonse zimene mungathe , simuyenela kukaikila kuti Yehova akukuyang’anilani ndipo adzakuthandizani kuti mupilile . — Sal . Ine n’nabisala ku cimtengo cakugwa . Kodi mungakonde kukatumikilako ku gawo laconco ? Monga otsatila a Yesu , timaidziŵa bwino nchito imene Mulungu watipatsa . Popeza angelo saoneka , sitingadziŵe kuti Mulungu amawaseŵenzetsa kufika pati pothandiza anthu pa zocitika zosiyana - siyana . M’bale wina wacicepele , dzina lake Henri , cinamuŵaŵa kwambili mu mtima pamene abululu ake anasiya coonadi , kuphatikizapo atate ŵake , amene anali mkulu wodziŵika . Kodi n’ciani cidzacitikila anthu amene amakana Yesu Kristu kukhala Mfumu yao ? Patapiza zaka , mkazi wa m’baleyo anabatizika n’kukhala wa Mboni za Yehova . Kuonjezela apo , ngati kholo limapatsa mwana mwamsanga ciliconse cimene wapempha , khololo limakhala ngati kapolo wa mwanayo . Kumbukilani kuti “ ana sayenela kusunga cuma kuti cidzathandize makolo awo mtsogolo , koma makolo ndiye ayenela kusungila ana awo . ” — 2 Akor . Abulahamu ndi banja lake anasiya nyumba yao ndi acibale ao ena ku Uri , mzinda wotukuka wa ku Mesopotamiya . Komanso , masomphenyawa ni cilimbikitso cacikondi cocokela kwa Atate wathu wakumwamba . Kodi ndiye kuti Mike wayamba kusokonezeka ? ’ ” — Becky , wa ku California , U.S.A . M’kalatayi , Agiripa analemba zokhuza Yerusalemu kuti : “ Mzinda Woyela . . . si mzinda wa dziko la Yudeya cabe ai , koma ndi wa maiko ena ambili kuphatikizapo oyandikana nalo . Izi zili conco cifukwa cakuti maiko enawa akhala akulamulidwa ndi mafumu aciyuda . ” Njila yokha imene mungadziŵile , ndi kuseŵenzetsa Baibulo . Lemba la Malaki 4 : 2 limatitsimikizila kuti anthu amene adzacilitsidwa ‘ adzadumphadumpha ngati ana a ng’ombe amphongo onenepa ’ cifukwa codziŵa kuti amasulidwa ku ucimo . Anacita zinthu zoonetsa kuti anali ndi cikhulupililo colimba ngati thanthwe . ( Mac . Cifukwa cakuti Abulahamu anali kumvela Yehova ngakhale pa zinthu zing’onozing’ono , ubwenzi wake ndi Mulungu unalimba kwambili . Akhristu acicepele amakumana ndi zinthu zambili zimene zimafuna kuti akhale olimba mtima kuti akwanitse kutumikila Yehova . N’cifukwa ciani tiyenela kuyesetsa kuona zabwino mwa io monga mmene Yehova amacitila ? YEHOVA AMAONA ZABWINO MWA ATUMIKI AKE ( 3 ) Kodi aliyense wa ife angapindule bwanji ndi fanizo la Yesu limeneli masiku ano ? Mfumu ya nzelu Solomo inafotokoza kuti : “ Nzelu zimateteza monga mmene ndalama zimatetezela , koma ubwino wa kudziwa zinthu ndi wakuti nzelu zimasunga moyo wa eni nzeluzo . ” Pa zaka zonse 13 zimene Yosefe anakhala m’ndende , anaonetsa kuti anali kuona zinthu monga mmene Yehova amazionela . ( Gen . Pali cifukwa cina cimene cimatipangitsa kudziŵa kuti Ufumu wa Mulungu udzayamba kulamulila dziko posacedwapa . Anthu ocita zoipa m’dzikoli aipa kwambili . Zoonadi , ngati titengela Yesu , nthawi zonse tidzayamba kucita zinthu mwacikondi . Kodi Yehova anam’thandiza bwanji Mose kuti akwanilitse nchito yovuta ? Ngakhale anthu a m’banja langa amene si Mboni amakamba kuti ndikanafa kale cifukwa coseŵenzetsa mankhwala osokoneza bongo kapena pomenyana ndi anthu . Ndasangalala kuonananso ndi inu . ( c ) Kodi ndife otsimikiza kuti moyo udzakhala bwanji m’dziko latsopano ? 97 : 10 ) Mwacitsanzo , tifunika kudana ndi ciwelewele . Pokhala Tate , Yehova mwacikondi ndiponso mokoma mtima , anawapatsa malangizo omveka bwino . 10 , 11 . ( a ) Ni makhalidwe oipa ati amene amaonetsa kuti anthu sakonda anzawo ? Analudziŵa kuti zakudya n’zofunika . Ndiyeno anali kuupepeta asanaupele . Kupela ufa wokwanila banja lonse kunali kutenga maola ambili . Ifenso Yehova watidalitsa . Yehova amatsogolela na kudyetsa gulu lake la padziko lapansi kupitila mwa “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” Kapoloyo ali pansi pa utsogoleli wa Khiristu , “ mutu wa mpingo . ” ( Mat . 24 : 45 - 47 ; Aef . “ Sindinali kukonda zophunzila kusukulu , koma phunzilo la Baibulo linali losangalatsa kwambili . Mabanja ena amacita maseŵela ozikidwa pa zocitika za m’buku la Ekisodo . 6 : 33 , 34 ) Conco , muzikhala na umoyo wosalila zambili . Muziika zinthu zauzimu patsogolo osati zakuthupi . Kusoŵa ndalama ( Onani palagilafu 17 ) Ningawalimbikitse bwanji kuti azicita zinthu mogwilizana na malangizo a Yehova ? ’ Zimene mwanenazo zicitike ndithu kwa ine . ” — Luka 1 : 26 - 38 . Yesu anali woganizila ena ndi wacifundo . Masiku ano , zimenezi zitanthauza kuti ayenela kucotsedwa mumpingo . Iwo amakhulupilila kuti zomelazo zakhalako zaka masauzande ambili , mwina kuposa camoyo ciliconse padziko lapansi . Mfumuyo idzaukitsa anthu mamiliyoni ambili amene ali kumanda ndi kupanga makonzedwe akuti anthu oukitsidwawo aphunzitsidwe za Yehova . ( Chiv . Mu 1513 C.E . , wofufuza malo wina wa ku Spain , Juan Ponce de León anayenda ulendo wa panyanja m’zilumba za Caribbean n’colinga cofufuza mankhwala a moyo ochedwa kasupe wa unyamata . Mwina tili ndi zocita zambili m’nchito ya Ambuye , koma ndife olefulidwa cifukwa tikuona kuti utumiki wathu sukubala zipatso . ( 1 Akor . Ziphunzitso zimenezi n’zofunika kwambili , ndipo n’kutheka kuti ni zina mwa mfundo za coonadi zoyambilila zimene tinadziŵa titangoyamba kuphunzila Mau a Mulungu . Okalamba pamodzi ndi owasamalila , angacititse zinthu kukhala zosavuta ngati ali ndi maganizo oyenela . 1 : 8 . 22 : 3 ) Mkhristu angakhalenso pa ciyeso ngati wacoka panyumba n’kupita kwinakwake kutali kukacita bizinesi , kapena ngati amaseŵenza na munthu amene si mwamuna kapena mkazi mnzake . Ndiyeno ananipeleka ku kiliniki ya pakampu kuti akanipime ndi kuona ngati sin’nathyoke mafupa . Yelekezelani umoyo wao ndi wanu ndi mmene anali kumvela , ndi kuona zimene mukanacita mukanakhala io . Barber amene anali wokangalika anakamba kuti : “ Tinakwanitsa kulimbikitsa oyang’anila madela ocepa amene tinali nawo . Tinapitilizanso kufalitsa magazini ya Nsanja ya Mlonda mwezi uliwonse na kuitumiza m’dziko la Canada kumene inali yoletsedwa . Ndiyeno m’pempheni kuti muŵelenge naye limodzi la malonjezo amenewo m’Baibulo . Baibo imagwilizanitsa ‘ tsiku lomaliza ’ ndi ulamulilo wa Ufumu wa Kristu . Mwayi wina waukulu umene timapeza cifukwa ca kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova , ni cilimbikitso cimene amapeleka tikavutika maganizo . Citani zinthu mwanzelu ( 1 Yoh . 3 : 12 ) Yehova anayesa kum’thandiza Kaini mwa kumuuza kuti : “ Ukasintha n’kucita cabwino , sindikuyanja kodi ? Mwamuna na mkazi amene amalemekeza mfundo imeneyi amayesetsa kulimbitsa cikwati cawo . Conco , n’nadzifunsa kuti : ‘ Kodi nidzakwanitsa kukuka ? Kodi anthu ambili amaliona bwanji khalidwe laciwelewele ? Munthu waconco amasankha mau amene angathandize ena osati kuwakhumudwitsa . ( Miy . Thompson , Jr . , amene anali woyang’anila cigawo anapenda ziyenelezo zanga kuti aone ngati n’nali woyenelela kukhala wadela . Nthawi zina ndimakonza tumphatso tung’onotung’ono ndi kulemba kakalata kaciyamikilo . ” Komanso , timayamba kukhulupilila kwambili kuti “ Yehova ali pafupi ndi onse oitanila pa iye . ” N’nakumananso na ciyeso cina pambuyo pakuti navala “ umunthu watsopano . ” Conco , m’malo mofuna kuti azicita zinthu mmene ife timacitila , bwanji osangowalandila mmene alili ? — Ŵelengani Aroma 15 : 7 . Conco , Davide anaika mtima wake pa kuthandiza Solomo . Anam’thandiza kupeza zomangila zonse zofunikila . Mwanjila imeneyi , iye anaonetsa cikondi cimene Atate ake ali naco . Koma zofunika kuposa zonse ndi zinthu za kuuzimu , monga kuŵelenga Mau a Mulungu ndi kuwasinkhasinkha . Liu lacigiriki limene analimasulila kuti ‘ kufunafuna ndi mtima wonse , ’ limatanthauza kulimbikila . ( Mac . Adzacita ciani mtsogolo ? Ni mfundo iti yofunika imene imathandiza Akhristu kukhala ogwilizana ? Komanso , Baibo ni yocititsa cidwi pa nkhani yokambilatu za mtsogolo . — Onani bokosi yakuti , “ Kodi inatha nchito kapena imakambilatu zinthu zimene anthu akalibe kuzitulukila ? ” Tikapeza munthu wacidwi tiyenela kumulalikila uthenga wathu , koma sitiyenela kukhalitsa . 27 : 11 ) Pitilizani ‘ kukhutula za mumtima mwanu ’ kwa Mulungu mpemphelo . ( Sal . lingafunsidwenso kwa ife tikapita kukalalikila uthenga wa m’Baibulo kwa ena . “ Ndi bwino kudya zamasamba koma pali cikondi , kusiyana ndi kudya nyama ya ng’ombe yamphongo yodyetsedwa bwino pali cidani . ” imalimbitsa cikhulupililo cathu cakuti kuli Mlengi . Nthawi zina , nimacita kudzikakamiza kuti nikambe na abale na alongo mu mpingo wanga watsopano . Pamene izi zinali kucitika , atate anali atamwalila kale , ndipo amayi anali atabatizika n’kukhala Mboni ya Yehova . N’nakondwela pamene iwo ananiyankha kuti : ‘ Dokota wa ku Myanmar wodziŵa bwino za matenda a ubongo adzabwela kuno ku Japan posacedwapa . Ngati ndi conco , ndiye kuti muli ndi cinthu camtengo wapatali cimene ndi ubwenzi wanu ndi Mulungu . ( Genesis 12 : 10 - 20 ; 20 : 2 - 7 , 10 - 12 , 17 , 18 ) Zocitika zimenezi zinalimbitsa cikhulupililo ca Abulahamu . Mosakaikila , mkate wa ku Iguputo unali wokoma . 3 : 5 ) Komabe , n’zosatheka kuwapewelatu anthu aconco . 16 : 32 ; 17 : 27 ) Komanso , ngati muli na wacibale wocotsedwa , mufunika kukhala wodziletsa kuti musamakambe naye mosafunikila . Lamulo limeneli linalembedwa pa mitima yathu ndipo limatitsogolela kulikonse kumene tingakhale . Nanga , n’cifukwa ciani anthu ena amaona kuti mapemphelo ao sayankhidwa ? Ndithudi , kulakalaka zaciwelewele kungaononge ubwenzi wathu ndi Yehova . — Ŵelengani Yakobo 1 : 14 , 15 . N’zoona kuti mautumiki amenewa ndi okondweletsa . SIKUDZAKHALANSO NJALA Iyai . ( Luka 18 : 1 - 3 ) Ngakhale kuti woweluza ameneyu poyamba anali kukana kumthandiza , potsilizila pake anati : “ Ndicita zimenezi kuti asapitilize kumangobwela ndi kundisautsa kwambili , cifukwa mkazi ameneyu akundivutitsa mosalekeza . ” Mwacitsanzo , ganizilani mmene Yehova anacitila ndi Anineve m’nthawi ya Yona . Yehova amatikonda monga ana ake , ndiye cifukwa cake amatipatsa cilango ndi kutiumba mwacikondi Kodi khungu lake limamucititsa kulephela kudziŵa zonse zimene zikucitika pamalo pamene ali ? ( Yoh . 1 : 18 ) Kodi kuli munthu aliyense — wasayansi kapena wina — amene anaonapo camoyo cina cikusandulika n’kukhala ca mtundu wina ? Kulimba mtima kwa Mboni za Yehova pankhani yosatengako mbali m’nkhondo , kwathandiza anthu masauzande ambili padziko lonse kudziŵa kuti Mboni zili ndi cikondi ceniceni pa Mulungu ndi pa anthu . M’nyengo yotentha ku Isiraeli , nthawi zina mvula sikugwa kwa miyezi ingapo . Ndi kulambila kotani kumene Yehova sakondwela nako ? Pa nthawiyo , Rehobowamu anali ataopseza anthu kuti adzawalanga “ ndi zikoti zaminga . ” Conco , mwina anali kudzifunsa kuti , ‘ Kodi anthu adzaniona bwanji nikapanda kuwalanga opandukawa ? ’ ( a ) Kodi anthu othaŵa kwawo amafunika zinthu ziti ? Ndinayamba kukonda kuŵelenga nkhani zokhudza amishonale kenako ndinayamba kuganizila zoonjezela utumiki wanga kwa Mulungu . ” “ Nimayesetsa kuona ngati mwana wanga walakwitsa zinthu mwadala , kapena wangocita zinthu mosaganiza bwino . Ena mwa anthu amenewa sanali a msinkhu wanga kapena a cikhalidwe colingana ni canga . 19 : 35 . Kodi tiyenela kuiona bwanji mfundo yakuti munthu angakhale na cimwemwe olo kuti satumikila Mulungu ? Mulungu adzaseŵenzetsa Yesu kuti acotse mavuto onse amene Mdyelekezi amacititsa . — 1 Yohane 3 : 8 . M’malomwake , afunika kukhala acikondi , aulemu , ndi oganizila ena . Masiku ano , anthu ambili amakana kumvetsela uthenga wabwino wa Ufumu umene ulalikidwa pa dziko lonse lapansi , kupeleka umboni ku mitundu yonse , dongosolo la zinthu lino lisanathe . ( Yobu 1 : 6 ) Ndipo ni mabuku atatu cabe a m’Malemba Aciheberi amene amachulako dzina lakuti Satana , limene limatanthauza “ Wotsutsa . ” Mabuku amenewa ni 1 Mbiri , Yobu , na Zekariya . Yehova anauza Mwana wake kuti : “ Khala kudzanja langa lamanja kufikila nditaika adani ako monga copondapo mapazi ako . ” — Sal . Kodi Yesu anaonetsa bwanji za nthawi pamene ulosi wake udzakwanilitsidwa ? NYIMBO : 127 , 118 Izi zimaphatikizapo kuwakhululukila akatilakwila . Kodi mungadzipeleke kuti mukathandizile m’maiko osoŵa ? Kusamvela kwa Adamu kunabweletsa mavuto aakulu . ( Gen . 9 : 28 ) Ndithudi , Nowa ni citsanzo cabwino ngako pa nkhani ya kukhala munthu wacikhulupililo na womvela . ( Salimo 115 : 3 ) Yehova amacita zinthu zimene aona kuti n’zofunika kucita osati cim’citila . Ponena za abale amene anasonkhanawo , mmodzi wa oyang’anila sitediyamuyo anati : “ Ili ni gulu la anthu a khalidwe labwino kwambili limene sin’nalionepo n’kale lonse m’sitediyamu ino . ( a ) Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti anatengela Atate ake ? Kodi iye caposacedwa anapeleka ndemanga yabwino komanso yocokela pansi pa mtima ? Koma olemba nchito ambili anakana kundilemba . 11 : 33 , 34 ; Dan . Ngakhale m’banja , tikhoza kukumana ndi mavuto amene angayese cikhulupililo cathu mwa Yehova ( Onani ndime 14 mpaka 16 ) Mwacitsanzo , zimakhala zovuta kwa anthu ena kukumbukila zonse zimene a dokotala angawauze pambuyo powapima . Apempheni kuti akambe maganizo awo , kuphatikizapo zilizonse zimene amakaikila . Kuyandikila Mulungu m’pemphelo , ndi kulimbitsa cikhululipilo pa malonjezo a m’Baibulo a m’tsogolo , kumathandiza Paul , Janet , ndi Alona kulimbana ndi nkhawa . Komanso , mtumwi Paulo anacenjeza Akhristu anzake za zinthu zimene zikanawalepheletsa kukalandila mphoto . N’naganiza kuti abale oyang’anila pa Beteli anali kufuna kuti nithandizeko nchito kwa nthawi yocepa cabe , koma zinthu sizinakhale conco . Kuwonjezela apo , Baibo ionetsa kuti atumiki acikhristu ambili a m’zaka 100 zoyambilila , kuphatikizapo mtumwi Petulo , anali okwatila . ( Ŵelengani Mateyu 6 : 22 , 33 . ) Mwa kubeleka ana , dziko lapansi linali kudzakhala paladaiso wodzala ndi anthu angwilo , ndipo anali kudzayang’anila zamoyo zonse . — Gen . Iye mwini adzalimbana ndi anthu onse powaweluza . Kumacepetsa nkhawa , nkhanza , na kupanikizika maganizo Mulungu anati : “ Musabe , musanamizane ndipo aliyense asacitile mnzake cinyengo . ” Mwacitsanzo , atumiki othandiza amaonetsetsa kuti tili ndi zofalitsa zokwanila zimene tidzagwilitsila nchito mu ulaliki , ndiponso amalandila alendo amene amabwela ku misonkhano . Iye anaona kuti mbali yakuda ya maso imene imazungulilidwa ndi mbali yoyela ya maso a bwenzi lakelo , ndi yokongola kwambili ngati njiwa zimene zikusamba mumkaka . Yehova amawafunila zabwino atumiki ake , ndipo iye sanasinthe maganizo pankhani yokhudza cikwati . ( Yesaya 65 : 11 ; Akolose 3 : 5 ) Conco , n’naleka kuchova njuga . Conco , timayamikila ngati ena amalemekeza nthawi yathu mwa kukamba nafe mwacidule . Koma kodi vuto lawo linali ciani ? Mu 2014 , Stephanie anamanga banja ndi Aaron , ndipo pano tikamba , atumikila pa Beteli ku Ghana . Ndithu ndikuthandiza . ” ( Yes . 41 : 10 ) Tikatelo , ubwenzi wathu na Yehova umalimba . Citsanzo ca m’Baibulo ca banja la Yakobo cikuonetsa kuipa kwa kukwatila mitala . Iye anapeleka uphungu wamphamvu ku mipingo ina ya m’cigawo ca Asia Minor . Kodi anaupeleka motani ? 13 : 5 , 13 ) Komabe , Baranaba anaona zabwino mwa Maliko osati zofooka zake . ( 2 Timoteyo 3 : 16 ) Kodi Baibo imatiuza ciani ? Komabe , Yosefe sanalole zofuna za mkaziyo kapena kulola kuti azimukopa . Dziŵani kuti zocita zanu zimakhudza kwambili ana anu Tanena izi cifukwa Yesu anakamba kuti ngati wocimwa salapa pambuyo pakuti m’bale wake wakambilana naye , waitananso mboni , ndiponso abale a maudindo , ayenela kuonedwa monga “ munthu wocokela mu mtundu wina komanso ngati wokhometsa msonkho . ” Kwa zaka zambili , Yehova wakhala akusankha amuna kuti atsogolele . ( Ŵelengani Salimo 102 : 19 - 21 . ) Cimodzi mwa zitsanzo zimenezi cikupezeka pa Agalatiya 4 : 21 - 31 . Pa intaneti si malo abwino ‘ olangizila mofatsa anthu otsutsa . ’ ( 2 Tim . 2 : 23 - 25 ; 1 Tim . Aaron na Stephanie Pansi pa mikhalidwe yabwino , anthu anafunikila kufutukula Paladaiso mpaka dziko lonse lapansi . Zioneka kuti Akristu ena mumpingo wa kumeneko anapatsidwa mwai wokhala nzika za Roma . Cifukwa cakuti anakhala nzika anali ndi mwai wocita zinthu zina zimene abale ena sanaloledwe kucita . Phale limene panalembewa dandaulo la munthu wina woseŵenza m’munda Komanso , tikakhala mabwenzi a Yehova , m’pamene timaona kuti umoyo wathu uli na phindu . — Mlal . Tingaonetse bwanji kuti ndise odzicepetsa ndi ofatsa ? Musaiŵale kuti “ Yehova amadziŵa kupulumutsa anthu odzipeleka kwa iye akakhala pa mayeselo . ” Olo zinali conco , n’tafika zaka 14 , n’nabatizika mu kamtsinje kapafupi . Ananimiza katatu , monga cizindikilo ca Utatu . Bungwe Lolamulila limapeleka malangizo amene timalandila m’zofalitsa zathu , pamisonkhano ya dela ndi ya cigawo . ( Yak . 2 : 23 ) Panthawi imeneyo muyenela kuti munadziŵa kuti mwapeza cinthu camtengo wapatali kuposa golide . Zina mwa mfundo zimene Oweluza a Isiraeli anapatsidwa ndi izi : Olo zinali conco , anakwanitsa kupezekapo pa nthawi ya imfa ya Yesu . ( Yoh . Buku linanso limati : “ Atsogoleli acipembedzo analibe mphamvu yolimbikitsa anthu kucita zabwino ndipo ambili a io sanafune kucita zimenezo . Khulupililani uthenga wabwino ! ’ ” Yesu anagwilitsila nchito fanizo limeneli cifukwa abusa ndiponso ziweto zinali zinthu zimene anthu a ku Isiraeli wakale anali kuzidziŵa bwino . Panthawiyo , Akristu ena okhulupilika adzakhala atadzozedwa . Motelo , n’zoonekelatu kuti si canzelu kutengela acinyamata amene amapatuka n’kuyamba kucita zinthu paokha . Ndi zinthu zitatu ziti zimene zatithandiza kulalikila uthenga wabwino ? Kodi odzozedwa ayenela kudziona bwanji ? Mau ake amafanana kwambili na mau ali m’Baibo masiku ano ( a ) Ni makhalidwe abwino ati amene Danieli anaonetsa ? Kodi muganiza kuti anthu amene anapanga makinawo akanakwanitsa kuwapanga ngati sanagwilizane pa pulani limodzi ? 2 : 11 - 14 ) Koma sanataye mtima . M’maŵa patsikulo , mkulu wa ansembe anapeleka nsembe pa kacisi monga mwa nthawi zonse . Iye anakamba kuti : “ Zinali zovuta kuvula umunthu wanga wakale . Kumbukilani kuti Yesu anakamba kuti iye ndi “ njila , coonadi ndi moyo . ” PAMENE tiphunzila Baibulo ndi anthu , nthawi zambili timaphunzila nao buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceniceni , n’colinga cakuti tiwathandize kudziŵa Yehova ndiponso coonadi ca m’Baibulo . Pali acicepele ambili m’mipingo yonse ya Mboni za Yehova pa dziko lapansi , amene tiyenela kuwayamikila na mtima wonse . Iye anati : “ N’naona monga kuti angelo anacititsa khungu asilikaliwo ndipo Yehova anatipulumutsa . ” — Sal . Amenewa ndi maganizo abwino amene tiyenela kukhala nao . Conco lengezani , lengezani , lengezani Mfumu ndi ufumu wake . ” Kupeza Citonthozo pa Nthawi Yovuta 6 Mu 1982 , m’dziko la Sierra Leone , abale odzipeleka anagwila nchito mwakhama . Iwo anakonza malo ndi kumangapo kafiteliya pogwilitsila nchito zipangizo zimene anali nazo . Kodi mfundo imeneyi ionetsa kuti anthu atsala pang’ono kuthetsa mavuto amene awasautsa kwa nthawi yaitali ? 1 : 28 ) M’malomwake , iye anasankha kulumpha malile amene Mulungu anamuikila akuti asadye cipatso coletsedwa . Poyankha , Petulo anati : “ Inde Ambuye , inunso mukudziŵa kuti ndimakukondani kwambili . ” ( Yoh . Zimathenga nthawi kuti onse asinthe maganizo ao . Napindula Cifukwa Coyenda ndi Anthu Anzelu ( W . ( b ) Nanga ise tingakhale otsimikiza za ciani ? Ngakhale kuti mipukutu yoyambilila ya Baibulo palibe , tingatsimikizile kuti Mabaibulo amene tili nao ni olondola mwa kuwayelekezela ndi makope ndiponso mipukutu yakale ya Baibulo . 21 : 1 - 3 , 6 , 7 . M’malomwake , amene anali kudwala matendawa , anali ndi udindo wodziŵitsa ena kuti ali na khate . — Levitiko 13 : 45 , 46 . Conco , n’naganiza zopita kukakamba naye ngakhale kuti zinali zovuta . Iye anandithandiza kusamalila amai mpaka pamene iwo anamwalila . Zinthu zinafika poipa cakuti ‘ anthu oipa anali kupondeleza anthu olungama . ’ KULANGA MOYENELA Nthawi zonse Yehova amatilanga “ pamlingo woyenela . ” Mofanana ndi mmene ana ambili amamvelela akakhala kutali ndi makolo ao , Jimmy anaona kuti sanafunikilenso kukonda ndi kumvela amai ake . — Ŵelengani Miyambo 29 : 15 . Nthawi zina ana amamasuka kufotokoza za kukhosi pamene acitila zinthu pamodzi na makolo awo , osati kucita kukonza nthawi yokambilana nawo . Ngakhale kuti zinthu zina za m’masomphenya amenewa n’zophiphilitsa cabe , zingakuthandizeni kudziŵa amene ali kumwamba ndi mmene zocita zawo zimakukhudzilani . Conco , tizikhala womasuka kupemphela kwa Mulungu ndi kum’fotokozela zonse zokhudza cisoni cimene tili naco . Paulendowo iye anatenga Timoteyo ndi Tito ndi kupita nao ku Efeso , kenako ku Kerete ndipo mwina anakafika ku Makedoniya . ( 1 Tim . Iye anafotokoza Malemba momveka bwino cakuti khamu la anthulo linakhulupilila kuti Yesu ni “ Ambuye ndi Khristu . ” N’ciani cingatithandize kupewa misece ngati wina watilakwila mumpingo ? Mulungutu akudziŵa kuti tsiku limene mudzadye cipatso ca mtengo umenewu , maso anu adzatseguka ndithu , ndipo mudzafanana ndi Mulungu . Mwacitsanzo , ku Antiokeya wa ku Pisidiya , Paulo ndi Baranaba molimba mtima anauza Ayuda otsutsa kuti : “ Kunali koyenela kuti inu mukhale oyamba kuuzidwa mau a Mulungu . Timasangalala ndi cilengedwe cimeneci cifukwa mwacibadwa timakwanitsa kuzindikila zinthu zokongola . — Ŵelengani Salimo 19 : 1 ; 104 : 24 . 9 : 4 ) Mosakaikila , tiyenela kuona magazi monga mmene Mulungu amawaonela , ndi kumvela lamulo lake lakuti tiziwapewa . Mulungu amationa kuti ndife ofunika aliyense payekha . ( Genesis 1 : 26 - 28 ) Koma n’zacisoni kuti anataya zonsezi mwa kusankha kusamvela Mulungu , ndipo anakhala ocimwa . Mfundo yake inali yakuti iye anadziona wacabe - cabe monga fumbi ndi mafupa a makolo ake akufa . 7 : 10 , 11 ) Inde , ngati munthu acita khama kuti aleke kucita macimo , zimaonetsa kuti anaipidwadi na chimo lake , ndi kuti amayamikila cifundo ca Yehova . ( Ŵelengani Yesaya 12 : 5 . ) Conco , musanabatizidwe mufunika kudziŵa tanthauzo la kudzipeleka kwa Mulungu . 102 : 17 ) Dalilani lonjezo limenelo . Kwa za 1000 , Yesu ndi olamulila anzake adzathandiza anthu kukhalanso angwilo . — Chiv . ( 2 Timoteyo 3 : 1 - 5 ) Akristu amene akufuna kuthetsa khalidweli , angacite bwino kuganizila citsanzo ca m’Baibulo ca mkazi wakaleyu , amene anali kuthamangathamanga ku citsime kukatunga madzi . ( Deut . 33 : 13 , 17 ; 1 Maf . kuona kuti citamando cimeneci cimakwela kwa Yehova na Yesu caka ndi caka pa mwambo wa Cikumbutso . 4 : 9 , 10 ) Dipo ndi mbali yofunika ya uthenga umene timalalikila , ndipo odzozedwa amatsogolela pa nchito yophunzitsa anthu ponena za dipo limeneli ndi mmene lingawapindulitsile . ( 1 Akor . Mwacitsanzo , ngati mufuna , mungasamukileko ku mpingo wosoŵa . Anali kudela nkhawa kwambili za umoyo wawo wauzimu , ndipo anali kudzipeleka na mtima wonse pofuna kuwathandiza . Iwo anali kudzimva kuti ali pa mtendele ndiponso otetezeka . Tikamalalikila timalimbitsa cikhulupililo cathu cifukwa cakuti timakumbukila malonjezo a Mulungu ndi mfundo zake zabwino Iye anacita cidwi ataona kukongola kwa nyumbayo ndi maluwa ake ndiponso atamvetsetsa colinga cake . ( Yak . 4 : 8 ) Ngati timakonda kwambili Yehova , timayesetsa kumukondweletsa mwa zocita ndi zoganiza zathu . Citsanzo ca Amosi cionetsanso kuti Yehova amaona zimene atumiki ake angathe kucita . Anthu ambili anali kuona Amosi kuti sanali wofunika kwenikweni . Pambuyo pake , abalewo anafotokozela Arthur kuti pokwela pamtenjepo , anaseŵenzetsa makwelelo , ndiyeno makwelelowo anacotsedwapo . Conco , Akristu naonso anali kugwilitsila nchito zombo poyenda m’madela ambili . • “ Njila zake zonse [ Mulungu ] ndi zolungama . Malemba amaonetsa kuti anthu ena ochulidwa m’Baibulo anali kuimila cinthu cina cacikulu codzacitika mtsogolo . ( Mat . 22 : 37 - 39 ) Kukonda Yehova ndi mfundo zake , kudzatithandiza kukonda munthu mnzathu . M’nkhani yotsatila tidzaphunzila mmene tingacitile zimenezi . [ Cithunzi papeji 10 ] Timakhala ofunitsitsa kumva maganizo ao ndi kukhala ololela ngati pakufunika kutelo . — Afil . PAMENE ndinali ndi zaka 9 , ndinaleka kukula . Posapita nthawi , tinayamba kuphunzila kaŵili pa mlungu ndipo phunzilo lililonse linali kutenga maola aŵili . Zina mwa ziphunzitso zimenezo zinali zocokela kwa anthu akunja aja , Aristotle na Plato , amene anakhalako Yesu Khiristu asanabadwe . ( Ŵelengani Yohane 15 : 11 ) Ndipo iye anatitsimikizila kuti cimwemwe cake cidzakhala mwa ise . ( Salimo 34 : 7 ) Mwacitsanzo : Ndiyeno , iye anali kuyang’anitsitsa Rabeka pamene anali kuthamangathamanga ndi mtsuko wa madzi kuti adzaze comwelamo ziŵeto . — Genesis 24 : 20 , 21 . Ena a iwo anatipempha magazini . ” Timacita kusoŵa nthawi yowaphunzitsa . ” Abale na alongo anali kudziŵa kuti apolisi anali kutilondalonda . Tengelani Citsanzo Cao — ‘ Tamvelani Maloto Awa ’ 10 Ndiyeno , cikhulupililo cake cinayamba kufooka . Nanga n’ciani cinalakwika ? 2 : 15 ) Kodi tingakulitse bwanji luso la mmene timaseŵenzetsela Mau a Mulungu ? Cifukwa cakuti Abulahamu anali wokhulupilika ndi womvela , Yehova anacita naye pangano pamene anati : “ Ine ndidzatulutsa mtundu waukulu mwa iwe . Ndidzakudalitsa . ” ( Gen . COLINGA : Kutsimikizila kuti Mfumu Mesiya adzabadwila mu mzele wa Davide ndi kuti zimene Ufumu udzacita zidzakhala kwamuyaya Onani kabokosi kakuti “ Kufanana Pakati pa Fanizo la Matalente ndi la Mina . ” Mcitidwe wodzikuza umodzi wokha , unataitsa mneneli wosatomolewa dzina uja , moyo wake ndi ciyanjo ca Yehova . ( Mac . 20 : 35 ) Mwa mau na zocita zathu , tingathandize ana athu ndi acatsopano kuona mmene angacilikizile pa nchitoyi , kuti nawonso alandile madalitso . Mwacidziŵikile , Yehova na Yesu amaona anthu amene amayesetsa kuti akapezeke pa msonkhano wofunika kwambili umenewu wa pa caka . Kodi mumakamba naye mokwanila Yehova ? Koma masiku ano , tingamvetsetse bwinobwino tanthauzo la maulosiwo . Iye anaphunzitsa coonadi ana ake 6 , ndipo anapitilizabe kupezeka pamisonkhano yampingo ndi ikuluikulu . Mavuto amaculuka , koma citonthozo cimasoŵa . Ngati ‘ tiyembekezela ’ Yehova ndi ‘ kum’dalila ’ mwa kum’pempha nzelu ndi citsogozo , ndiponso ngati titsatila malamulo ake ndi mfundo zake , “ iye adzacitapo kanthu . ” ( Sal . Kupanda cilungamo kwake ŵati ! Kodi mgwilizano wa Timoteyo na mtumwi Paulo utiphunzitsanji ? Analinso kuukitsa akufa . Nyuzipepalayi inafotokozanso kuti ciŵelengelo cimeneci ndi “ 3 lotsatilidwa ndi mazilo 23 kapena kuti 3 tililiyoni kuwilikiza nthawi 100 biliyoni . ” Coyamba , tiyenela kuyesetsa na mtima wonse kusakila anthu ‘ amene ali ndi maganizo abwino amene angawathandize kukapeza moyo wosatha . ’ Ndipo izi ndi zimene Mboni za Yehova zimakhulupilila . Eliya atakumana ndi Ahabu anamuuza mosapita m’mbali kuti ndi wakupha ndi wakuba . Kumeneko , anthu amene ana athu anawathandiza kuphunzila za Yehova , anali kuyamikila kwambili . Koma zoona zake n’zakuti Timoteyo anasankha kupita . Kucita daunilodi zofalitsa pa mawebusaiti ena , kupatulapo ya jw.org , kungationonge mwauzimu . Linali tsiku limene sindidzaiŵala . Ifenso tikumenya nkhondo yoopsa ndi yolemetsa . Ndi umboni wotani umene tili nao woonetsa kuti Yehova wathandiza anthu ake kuteteza ufulu wao wolalikila ? Robert sanali kudziŵa vuto limene anali nalo mpaka pamene analoŵa m’cikwati . Tikacita zimenezo tidzaona kufunika kwa pemphelo , monga mmene nkhani ino ifotokozela . Conco , kudzipatulila kwa Yehova kumaphatikizapo zambili , osati kungolonjeza kuti tidzacita cifunilo cake na kubatizika . ( b ) Ndi makonzedwe ati acikondi amene athandiza kuti Nyumba za Ufumu zimangidwe m’madela amene mipingo ilibe ndalama zokwanila zomangila Nyumba za Ufumu ? 4 : 12 , 13 . “ Ndakweza maso anga kuyang’ana inu , kuyang’ana inu amene mukukhala kumwamba . ” — SAL . Delphine anati : “ N’napemphela kwa Yehova kuti anithandize kupeza zocita zimene zinganitonthoze . ” Iye akayang’ana kacizindikilo , kompyutayo imatulutsa mau akuti , “ Ciyembekezo cimene cili m’Baibulo ndi cakuti dziko lapansi lidzakhala paladaiso pamene sikudzakhala kudwala kapena kufa , Chivumbulutso 21 : 4 . ” ( b ) Tifunika kucita ciani kuti tikhale na ufulu wocokela kwa Yehova ? Conco , tifunika kuvomela ciitano na mtima wonse na kuyamikila zilizonse zimene otiitanawo atikonzela . Koma kodi anthu amene ali ndi ciyembekezo codzakhala ndi moyo kosatha padziko lapansi adzasangalala nao pa cikwati cimeneci ? Tingatsimikize bwanji kuti Mulungu afuna kuthetselatu nkhanza ? Iwo amakana kuti Yesu ndi Kristu kapena kuti Mesiya ndipo amasokoneza ubale umene ulipo pakati pa Mulungu ndi Mwana Wake , Yesu Kristu . Tifunikila kukhala paubale wabwino ndi Mlengi wathu . Magazi a Yesu anakhetsedwa pamalo ena amene anali kunja kwa Yerusalemu ochedwa Gologota , “ kuti macimo akhululukidwe . ” Kodi zimenezi zikusonyeza ciani ? Ndipo n’kosagwilizana ndi Malemba . Pambuyo pa zaka 500 , Yesu Kristu nayenso anali kugwila nchito yophunzitsa imeneyi . Safuna kutaya ulamulilo . Podzafika mu 1922 , panali ofalitsa Ufumu acangu oposa 17,000 amene anali kulalikila m’maiko 58 padziko lonse lapansi . Koma Akristu okhulupilika anapulumuka cifukwa cakuti anamvela malangizo a Yesu . Woyang’anila dela ndi mkazi wake akamacezela mpingo wathu , tikhoza kuwaitana kunyumba kwathu ngakhale kuti sitiwadziŵa bwino . Buku lina linati : “ Pa mphamvu 5 zimene munthu ali nazo , mphamvu ya kumvela ndiyo imatsilizila kutha . Si kuti iye ni Mlengi wamphamvuyonse cabe , koma alinso Atate wathu wokhulupilika ndi Mnzathu . Yehova Atamandike Cifukwa ca Kudzipeleka Kwanu ! Posacedwa , pa Aramagedo , Yesu adzathetsa ulamulilo wa Satana , na kuwononga onse amene ali kumbali ya Mdyelekezi . Yesu anali kutsitsimula anthu opanikizika , kulimbikitsa ofooka , ndi kutonthoza anthu ovutika maganizo . ( Luka 12 : 32 ) Ciŵelengelo cao ndi cocepa poyelekezela ndi amene adzakhala padziko kosatha . — Ŵelengani Chivumbulutso 7 : 4 , 9 , 17 . Mwana wa Mulungu . ” M’bale wina wodzozedwa amene watumikila mokhulupilika kwa zaka zambili anati : “ Ndangomaliza kumene kuŵelenga buku la Yobu m’Baibulo lokonzedwanso , ndipo ndikuona kuti kwa nthawi yoyamba , ndi pamene ndalimvetsetsa . ” Magaleta na okwelapo ake anatumiwa kumadela osiyana - siyana a dziko lapansi . KUKONZEKELA N’KOFUNIKA 3 : 8 ) Kodi tingawapatse ndalama zowathandiza pakagwa za mwadzidzidzi kapena kuwathandiza kuti apeze nchito ? Kwa zaka zambili , Yehova analosela kuti adzasankha mtsogoleli wapadela wa anthu ake . N’cifukwa ciani tifunika kuyembekezela Yehova na mtima wonse kuti adzakwanilitsa malonjezo ake ? ( Aroma 6 : 21 ) Koma lomba anasintha , mofanana ndi Akorinto amene Paulo anawalembela kalata . Kudalila Mulungu n’kofunika kwambili , osati cabe pamene wacibale wanu wadwala mwakayakaya , koma ngakhalenso pamene muli na cisoni wodwalayo akamwalila . Ralph Walls Koma Rose ataphunzila Baibo , anadziŵa kuti coonadi conena za Ufumu wa Mulungu n’camtengo wapatali . ( Onani palagilafu 11 - 14 ) Kodi Yehova amationetsa bwanji kuti amatikonda tikalakwa ? 7 : 8 ) Anchito odzipeleka amenewa ndi okondwa kutengako mbali pa nchito ya anthu a Yehova masiku ano . ( Luka 22 : 20 ) Nkhani ya pa Mateyu imagwila mau a Yesu ponena za vinyo kuti : “ Vinyoyu akuimila ‘ magazi anga a pangano , ’ amene adzakhetsedwa cifukwa ca anthu ambili kuti macimo akhululukidwe . ” — Mat . KULEZA MTIMA Mwacitsanzo , mu 1995 , n’napatsidwa nchito yophunzitsa abale m’Sukulu Yophunzitsa Utumiki . Mwacikondi , anali kuganizila zosoŵa za anthu zauzimu , zakuthupi , ndi mmene anali kumvelela . Anthu sanalengedwe kuti azicita zoipa , kudwala kapena kuti azifa . Tidzaphunzilanso mmene tingaphunzitsile cikumbumtima cathu ndi mmene tingacigwilitsile nchito popanga zosankha zanzelu . Coyamba , panacitika civomezi camphamvu . Kodi Malemba amatilangiza kucita ciani ponena za dzikoli ? Anthu ambili masiku ano akaŵelenga lamulo limene Yehova anapatsa Adamu , amaona kuti Adamu anamanidwa ufulu wocita zofuna zake . Anatelo kuti iyeyo alandile mpingowo uli wokongola ndiponso waulemelelo , wopanda banga kapena makwinya kapenanso ciliconse ca zinthu zotelo , koma kuti ukhale woyela ndi wopanda cilema . ’ ( Aef . 34 : 14 ) N’zoona kuti kucita zimenezi sikopepuka nthawi zonse . Mosiyana ndi Yehova ndiponso Yesu , ife sitingathe kuthetsa ngozi zacilengedwe , koma tili ndi mphamvu yocita zinthu zina . Mu 1939 , nkhondo yaciŵili ya padziko lonse itangoyamba , anawakakamiza kuloŵa usilikali ku German . Ndiyeno , m’pemphelo muyamikileni Yehova pa zinthuzo . Mtumwi Paulo anatengela citsanzo ca Yehova ndi Yesu . Yesu ndiye citsanzo cabwino koposa pankhani yophunzitsa ena kutenga maudindo aakulu . ( Luka 6 : 31 ) Ndiyeno , Alan adzifunsa kuti , ‘ Kodi ndimafuna kuti anthu azindicitila ciani ? ’ Ute David na Rachel ni zitsanzo ziŵili cabe zoonetsa mmene kuseŵenzetsa mfundo za m’Malemba ouzilidwa na kudalila mzimu wa Mulungu kungatithandizile kukhala mwamtendele ndi ena . Koma Uriya anakana kupita kunyumba kwake . Katswili wina wa Baibo anati : “ Malangizo amene anapelekedwa anali omveka bwino na osavuta kuwatsatila . Kuti ticite zimenezo tiyenela kukonzekeletsa maganizo ndi mtima wathu tsopano , kuti tikhale okonzeka kucita cabwino . Conco , tingaone kuti n’zosatheka kupambana pa nkhondoyi . Yehova Mulungu ndiye Kasupe wa moyo . Kuwonjezela apo , José anali kuvutika ndi opaleshoni ya khansa ndiponso mankhwala a mphamvu amene anali kumwa . Ngati n’conco , onani mau awa : “ Cinthu cimene unali kuyembekezela cikalepheleka cimadwalitsa mtima . Mwacitsanzo , mungaŵelenge pemphelo losonyeza kulapa limene Yona anapeleka pamene anali m’mimba mwa cinsomba . ( Salimo 90 : 10 ) Ndife oyamikila kwambili kuti Atate wathu Yehova watiphunzitsa mmene tingakhalile ndi moyo wabwino tsopano , ndipo watilonjeza tsogolo labwino kwambili . GANIZILANI nkhani iyi . N’ciani cingatithandize kutsanzila kukoma mtima kwa Mulungu ? Adamu na Hava atapanduka , Yehova anacita cinthu cacikulu kwambili coonetsa kuti ali na cikondi copanda dyela . Kuti tiziona zinthu mmene Yehova amazionela , tiyenela kusintha mmene timaonela anthu amene amaoneka ngati ofooka . Baibulo Limasintha Anthu Mau a mboni anali ofunika kwambili pofufuza . ( Onani bokosi lakuti “ Nchito Yofunika Kwambili . ” ) N’ciani cionetsa kuti Akhiristu a m’zaka 100 anaphunzila kucotsa cidani ? Iwo anali pa sitesheni ya sitima , makamela ali m’manja , kuyembekezela mlendo wapadela . 20 : 10 - 13 . Izi zitanthauza kulola maganizo athu kutsogoleledwa na mzimu woyela , kuti agwilizane ndi maganizo a Mulungu . Taganizilani nkhani ya Nowa . “ Ukucedwelanji ? Yaciŵili , nyama sizinalengedwe kuti zizikhala kosatha , koma anthu analengedwa kuti azitelo . “ Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba , ” 10 / 15 Conco , zinthunzi za Paulo m’zofalitsa zathu n’zogwilizana ndi maumboni ena akale okhudza maonekedwe ake . Ndipo ena zinthu zinali kuwayendela bwino m’dzikoli , koma anali kuonabe kuti cinacake cikusowa mu umoyo wawo . Ndine woyamikila kwambili kuti Yehova wanidalitsa ponipatsa mnzanga wokhulupilika ameneyu . Sanacitenso khama kuphunzila coonadi ponena za Mulungu , kapena nzelu zake . Koma , Yehova anauzila Debora kulosela kuti ulemelelo sudzakhala wa mwamuna aliyense . Iye anali kupeza zofunikila za mu umoyo wake mwa kugwila nchito yosoka zovala . Ndinapempha abwana anga kuti andilole kugwila nchito maola 60 m’malo mwa maola 72 . Kukambilana mfundo zimenezi kungatithandize kuona mmene tingakhalile ‘ olimba m’cikhulupililo . ’ — 1 Akorinto 16 : 13 . Kodi acicepelewo na makolo awo afunika kuganizila ciani popanga cosankha pa nkhaniyi ? Atapempha dalitso , Yesu anapatsila atumwi ake mkate wopanda cofufumitsa ndi kuwauza kuti : “ Eni , idyani . ” Koma m’bale wina waciyela anatikonkha . Iye anali wamkulu ndi wamphamvu kuposa ine na munthu winayo . ( Mateyu 12 : 34 ) Izi zitanthauza kuti zimene timakamba zimaonetsa zimene zili mumtima mwathu . Kodi kukhala oceleza kukanawathandiza bwanji ? Kucokela pa mapangano amene takambilana , taona mmene amagwilizanilana ndi Ufumu wa Mesiya . Taonanso kuti Ufumu umenewu ndi wozikika zolimba mwalamulo . Satana Mdyelekezi , amene poyamba anali mngelo wokhulupilika wa Mulungu , “ sanakhazikike m’coonadi ” ndipo anabweletsa ucimo m’dziko . Unali uthenga wosangalatsa kwambili . Nimayesa kulimbikitsako ena amene amamvela conco . Anafotokoza kuti : “ N’nadziŵa kuti masiku ano , lembali silitanthauza cabe kukhala na nyumba yeni - yeni . ( Ŵelengani Akolose 1 : 15 , 16 . ) Tsiku lina , pamene zinthu zinafika poipa kwambili , woyang’anila dela wathu , M’bale Neville Bromwich , anabwela kunyumba kwathu madzulo . Loti , mwana wamasiye wa m’bale wawo , ndiye anakhala monga mwana wawo . Ndipo mau ake ndi ziphunzitso zake zinatsitsimula omvela ake . Timayamikilanso kusintha kwina kumene kunapangidwa kokhudza mapulogilamu a pa msonkhano wadela ndi wacigawo . Ndi funso liti limene lingakhalepo ngati tayembekezela mapeto kwa nthawi yaitali ? Iye amatsimikiza kuti “ Wakumva pemphelo ” ndi amene anamuthandiza kuti zinthu zimuyendele bwino . — Sal . Olosela ena akadziŵa kuti anthu ayamba kuwakhulupilila , mwacinyengo amatenga ndalama zambili - mbili kwa makasitoma awo . ( Ŵelengani Mateyu 18 : 35 . ) Mwacitsanzo , m’bale Peter , atumikila kwa zaka zoposa 74 mu utumiki wa nthawi zonse . Kwa zaka 35 anatumikila pa nthambi ku Europe . Mosapeneka , Abulahamu anamuyang’ana Sara . A Yohane : Mutanthauza ciani ? Tingacite ciani coonetsa kuti tikuseŵenzetsa mwanzelu ufulu wathu ? 12 , 13 . ( a ) Kodi ife Akristu tili ndi colinga cotani ? 13 : 16 ; 1 Pet . Hezekiya anadalila Yehova ndi mtima wonse ngakhale pamene ufumu wamphamvu padziko lonse wa Asuri , unaukila dziko la Yuda ndi kuopseza kuti udzawononga Yerusalemu . Mulungu anakhululukila Davide cifukwa cakuti analapa moona mtima . Luso limene tili nalo lotha kuuza ena maganizo athu ndi mmene tikumvela ndi mphatso yapadela yocokela kwa Yehova . Angayese kubisa mkwiyo kapena cidani cake , koma m’kupita kwa nthawi maganizo oipa a mumtima mwake ‘ adzaululika mumpingo . ’ ( Miy . Cingaphatikizepo kukhala wokoma mtima na waubwenzi . Analekanso kunikambitsa . Ngakhale ngati angaone kuti bodza lake n’laling’ono , nanga bwanji za lamulo la Mulungu lakuti : “ Musanamizane ” ? Adzaika nkhosa kudzanja lake lamanja , koma mbuzi adzaziika kumanzele kwake . ” M’malo mocita zinthu mopupuluma , bwanji osayamba mwaganizilapo ? Popeza kuti Satana ndi wacinyengo , iye amanyengelela anthu kuti apandukile Yehova , Mulungu wacikondi . 3 : 12 . Zimenezi zionetsa kuti iye anali wodziŵa zinthu . Mwacionekele , anali kudziŵa bwino mmene zinthu zinalili mu Isiraeli , ndipo anadziŵanso za mitundu yapafupi cifukwa ca amalonda oyendayenda . Izi zacititsa kuti ikhale magazini imene ikufalitsidwa kwambili padziko lonse . Iwo amapatula nthawi yophunzila miyezo ya Yehova ndi kutsatila zimene amaphunzila . Akatelo , amaonetsa kuti amaopa dzina lake . Imakhutilitsa colaka - laka cathu copitiliza kukhala na moyo . Inatipatsa mwayi womasuka ku ucimo na imfa . 41 : 14 , 37 - 43 ; Mac . 7 : 9 , 10 . Fotokozani mmene kupanga zosankha zabwino kumakhalila ndi zotsatilapo zabwino mtsogolo . Yesu anati : “ Aliyense amene wasiya nyumba , abale , alongo , abambo , amayi , ana kapena minda cifukwa ca dzina langa adzalandila zoculuka kwambili kuposa zimenezi , ndipo adzapeza moyo wosatha . ” ( Mat . Conco , olo kuti nthawi zina timakumana ndi zolefula , timapilila . Colinga cake n’cakuti akhale Mkristu wokhwima . Analemba kuti : 4 : 4 ) Masiku anonso , anthu amene amatsatila mfundo za Mulungu amaonedwa kuti ndi okhalila . Koneliyo ndi banja lake anabatizika . Satana amadziŵa kuti malangizo a Yehova adzatipulumutsa . Iye amayesetsa kutisokoneza kuti tisawatsatile . Cifukwa cakuti pamene atsogoleli a mtundu wao anam’pempha kuti awathandize , anawathandiza mwamsanga . “ Inu Ndinu Mboni Zanga ” 19 : 8 . Kodi acicepele angacite ciani kuti akhale olimba mwauzimu ? Yehova amacititsa cilengedwe cake kukhala ciliconse cimene iye angafune . Popanda maudindo onse amenewa ndinadzimva monga ndataikilidwa cinthu cacikulu . 16 Kodi Mukukumbukila ? Timakhumudwa tikakumana ndi mavuto aakulu paumoyo , monga kusakhulupilika kwa mwamuna kapena mkazi wathu , matenda aakulu , imfa ya munthu amene timakonda , kapena mavuto ena amene tingakumane nao pambuyo pa ngozi yacilengedwe . Ponena za ulosi wokhudza masiku otsiliza Yesu anati : “ Anthu amitundu ina adzapondaponda Yerusalemu [ amene akuimila ulamulilo wa Mulungu ] , kufikila nthawi zoikidwilatu za anthu amitundu inawo zitakwanila . ” 19 : 9 , 10 . ( Salimo 83 : 18 ) Khalidwe lake lalikulu ndi cikondi copanda dyela . Kapena ndimangoganizila zamalonda ndi kupeza umoyo wabwino ? Kodi cipembedzo coona mungacidziŵe bwanji ? Yehova Mulungu akugwilizanitsa anthu ocokela m’zipembedzo zambili mwa kuwaphunzitsa coonadi komanso kukondana . * Anthu a m’cipembedzo ca Cishinto amaloledwa kusakaniza zikhulupililo . M’malo mwake , anapita pa shelufu ndi kutenga buku la cikatolika limene limafotokoza za kuloŵana m’malo kwa atumwi kuti ndikaŵelenge ku nyumba . Koma tiyeni tikambilaneko zina mwa zifukwa zimenezo . Coyamba , tiyenela kupenda mmene Yehova waonetsela cifundo ndi mmene anthu enanso aonetsela khalidweli . Nkhani ya kuuka kwa akufa sinali yacilendo kwa atumwi a Yesu , cifukwa anthu ena anaukitsidwapo io asanabadwe . Sin’nali kudziŵa kuti cingathetse vuto la kusankhana mitundu ni kuthandiza anthu kusintha mitima yawo . Komabe , posakhalitsa Ayuda otsutsa anafika ndi kuyamba kulankhula zoipa ponena za Paulo ndi Baranaba . 4 : 6 , 7 ; 2 Akor . Posacedwapa , m’bale wina dzina lake Timothy , amene anayamba upainiya ali wacicepele anati : “ Nimakondwela kutumikila Yehova mu utumiki wanthawi zonse cifukwa ni njila imene nimaonetsela kuti nimam’konda . Kuti athandize Ayuda ambili amene panthawiyo anali kukamba Cigiriki m’malo mwa Ciheberi , kuti amve “ malemba oyela . ” — 2 Timoteyo 3 : 15 . Mfundo zake zingathandize munthu kuwonjezela luso lake la kuganiza na kupanga zosankha zabwino . — Miyambo 1 : 1 - 4 . Mau otanthauza kuti “ kumbukilani ” angamasulidwenso kuti “ chulani . ” 15 , 16 . ( a ) N’cifukwa ciani ndinu otsimikiza kuti Yehova adzakuthandizani kuphunzitsa ana anu ? Ngakhale zili conco , iye amafuna kuti tiziseŵenzetsa cuma cathu kucilikizila nchito ya gulu lake . Conco , patapita caka , ndinabwelela kunyumba kukasamalila amalume anga , amene anali wansembe . M’zaka za m’ma 1900 zokha , anthu pafupifupi 100 biliyoni anafa pa nkhondo . Ndipo pakati pa anthu amenewa pali amuna , akazi , ndi ana opanda mlandu . kukhala na cidalilo cakuti Mulungu adzakutetezani ? Mwacionekele , munthuyo pang’onopang’ono anayamba kunyalanyaza mau a Yehova . Koma sangabise colakwaco kwa Mulungu , cifukwa iye anakambilatu kuti kawalala aliyense adzaululika . ( Aheb . Kodi kupenda mipukutu yakale ya Baibulo kwaonetsa ciani ? N’namanga banja ndi Bethel pasanapite caka cimodzi mu 1958 , ndipo tinapitiliza kucita upainiya mu El Dorado . Olo kuti Yehova ndiye anacha mkazi wokondedwa ameneyu kuti “ Mfumukazi , ” Sara sanayembekezele kucitilidwa zinthu monga mfumukazi . Zimenezi zinacitikadi , mkatewu wocokela kumwamba wooneka ngati ‘ tunthu topyapyala ndi tolimba koma tosalala ’ ngati mame , unali kugwa m’mawa mulimonse . Polembela Akhristu a ku Korinto , iye anati : “ Koma ineyo ndidzagwilitsa nchito zinthu zanga zonse ndipo ndidzadzipeleka ndi moyo wanga wonse cifukwa ca miyoyo yanu . ” ( 2 Akor . Ngati tigwilitsila nchito mau okoma , anthu angamvetsele uthenga wathu ndipo ungawafike pamtima . Banja lake linali lolemela cakuti linali ndi anchito , koma Rabeka sanaleledwe ngati mfumukazi . M’malomwake , anali kugwila nchito mwamphamvu . 16 : 3 , 4 ; 19 : 24 - 29 ) Ifenso nthawi zina tingacite bwino kusintha zosankha zathu . Anthu pafupi - fupi 14 miliyoni anacoka m’maiko awo . Komabe , n’zacisoni kuti io anasankha kumvela Satana , “ njoka yakale ija , ” ndi kucimwila Mulungu . ( Chiv . 12 : 9 ; Gen . Mlengi wa anthu ndi dziko lapansi afuna kuti mudziŵe kuti nthawi yakuti acitepo kanthu padzikoli yayandikila . 25 : 35 , 37 , 40 ) Zimenezo zinacitika kwa mtumwi Paulo , amene nthawi zina anasoŵa zakudya ndi zakumwa . — 2 Akor . ( Afilipi 2 : 4 ) Tikudziŵa kuti n’zosatheka kukhalilatu ndi thanzi labwino m’dongosolo lino . Koma kodi n’zotheka kuphonya kamvedwe pa zinthu zina zimene mumaŵelenga ? Pamene anaona Yesu ali wakhanda , iye “ analankhula za mwanayo kwa onse amene anali kuyembekezela cipulumutso ca Yerusalemu . ” — Luka 2 : 38 . Koma mufunika kukhala wokonzeka kumuyamikila akatsatila malamulo anu . Mwacitsanzo , ngati munabatizika muli wamng’ono , mosakayikila zokhumba zanu zidzayamba kusintha pamene mukukula . Pamene mwana wathu anakana , tinapwetekedwa mtima kwambili cakuti tinayamba kulila . Mofananamo , Atate wathu wakumwamba amayamikila utumiki wanu . Komabe , si zacilendo kwa anthu okwatilana kukumana ndi “ nsautso m’thupi mwao . ” ( 1 Akor . 4 , 5 . ( a ) N’ciani cimene tikuphunzilapo pa cozizwitsa coyamba ca Yesu ? ( Levitiko 11 : 27 ) Kodi Yesu apa anali kunyoza mayi wacigiriki ameneyu na anthu osakhala Ayuda ? 12 : 25 ; 17 : 17 . Ngati timadalila Yehova ndi maphunzilo ake , tingapeleke mayankho ogwila mtima . ( Akol . Tiyeni tikambilane zitsanzo zisanu . Conco , n’kofunika kupemphela kwa Yehova , ndi kufufuza kuti tikhale okonzekela kaamba ka zakugwa mwadzidzidzi . 13 : 2 - 4 ; 14 : 26 ; 2 Akor . 1 : 19 ) Mwacitsanzo , ena monga Silivano ( Sila ) , Maliko , ndi Luka anatumikilanso monga alembi . ( 1 Pet . Yesetsani kukambilana ndi ana anu ndi kuwaphunzitsa kukonda Yehova kucokela pansi pamtima . ( Luka 12 : 16 - 21 ) Yehova amakondwela ngati timacita zinthu zomusangalatsa . Rubén anati : “ Zaka zambili nakhala nikuvutika na maganizo odziona kukhala wosafunika . 12 , 13 . ( a ) N’cifukwa ciani sitiyenela kutaya mtima ndi zimene zikucitika m’dzikoli ? Cofunika kwambili si nthawi yathu , koma ya Yehova . Kodi cinthu cimodzi cofunika cimene tingacite potonthoza ena n’citi ? Pambuyo posamalila zosowa za banja , kugwila nchito yakuthupi , kusamalila maudindo a mumpingo , ndi kucita zinthu zina zofunika cisamalilo mwamsanga , mumaona kuti mulibe nthawi yokwanila yophunzitsa ena mumpingo . Ndikumbukila kuti pa nthawi imeneyo ndinamva ngati kuti ndili ku dziko lina . M’Baibo mulinso zitsanzo zoticenjeza za anthu amene anacita ciwelewele cifukwa ca kusadziletsa . George ndi Adria anafotokoza kuti nthawi yoyamba kusamukila ku Ghana , anamvela monga abwelela ku umoyo wakale kwambili . Koma kucita zimenezi n’kovuta . Iye anaphunzitsidwa zinthu zambili ndi Atate wake , ndipo anali kuyamikila kwambili zinthu zimene Mulungu anamuphunzitsa . MBILI YANGA : MNYAMATA WOKONDA NDEWO Kodi kukhulupililana ndi kudalilana m’cikwati canu zayamba kucepekela ? Atafika ku bwalo la ndeke , anauzidwa kuti ndeke siipita tsikulo koma idzapita maŵa lake . Apa m’pamene iye anapeleka pemphelo laciŵili . Mwacitsanzo , tica wa kusukulu safuna kuti ana ake a sukulu azipitilila zinthu zimene anawalangiza . Nayenso Yesu safuna kuti otsatila ake ‘ azipitilila zinthu zolembedwa ’ m’Malemba Oyela . — 1 Akorinto 4 : 6 . Timayesetsa kukhala ‘ oyela mumtima mwathu ’ mwa kuganizila zinthu zoyela , khalidwe labwino , ndi zinthu zotamandika . Iyayi . Iye ayenela kuti anali kudziŵa kuti amene adzatuluke m’nyumba n’kubwela kudzakumana naye angakhale mwana wake . Ndi pa zocitika zina ziti pamene tiyenela kusankha nthawi yabwino yokamba ? Nayenso mlongo Olinda mwacimwemwe anati : “ Madilaiva a basi anali kutikwezela manja , ndipo ena anali kukamba mokweza ali m’motoka yawo kuti , ‘ Mucita nchito yabwino ! ’ Kodi lembali litanthauza kuti Aisiraeli anathandizidwa ndi angelo pankhondoyo , kapena kunagwa miyala yocoka kumwamba ? Kodi tifunika kukhalabe na ciyembekezo cotani ? 31 : 16 ; 1 Akor . Mulungu wathu ndiye wacititsa kuti paradaiso wauzimu akule . 13 : 15 ; Luka 24 : 28 - 30 ) Kuitanila munthu ku cakudya kunali ngati kumupempha kuti ukhale naye pa ubwenzi ndiponso pamtendele . Conco , dzina lakuti Yehova lingatanthauze kuti “ Amacititsa Kukhala . ” Nsomba Nyengo ya Cikumbutso ndi nthawi yabwino yosinkhasinkha zimene Yehova ndi Yesu anaticitila . Jordan anati : “ Popeza tsopano nadziŵa zambili zokhudza a Russell , nimaona kuti ka mphatso kocepa kameneka ni kamtengo wapatali kwa ine kuposa kale . ” Pamene Yesu adzabwela mu ulemelelo wake cisautso cacikulu citatsala pang’ono kutha , iye adzasonkhanitsila odzozedwa okhulupilika kumwamba . ( Mat . 24 : 31 ; 25 : 10 ; 1 Ates . ( Gen . 10 : 8 - 12 ) Kodi Mfumu yamuyaya inacita ciani ndi mfumu yopandukayo imene inali kufuna kulepheletsa colinga ca Mulungu cakuti anthu ‘ adzaze dziko lapansi ’ ? TSAMBA 25 • NYIMBO : 107 , 63 Mfundo yakuti “ aliyense wodzikweza adzatsitsidwa , koma aliyense wodzicepetsa adzakwezedwa , ” inandithandiza kukhala mtundu wa munthu amene Yehova afuna . ( Mat . ( Machitidwe 15 : 29 ) Lamulo limeneli , limathandiza Mkristu kuzindikila kuti sayenela kulandila cithandizo ca mankhwala cimene ciphatikizapo kuikidwa magazi athunthu , kapena zigawo zinai zikuluzikulu za magazi . M’bale wina pofotokoza mfundo imeneyi , anafunsa kuti : “ Mukanakhala kuti mukulalikila ku nyumba ndi nyumba pamodzi na Yehova , kodi sembe mukamba mwekha cabe , kapena sembe mumulola iye kukamba ? ” Cinanso , muyenela kuganizila nthawi na malo kumene mungakumane na ziyeso ndi kuonelatu zimene mungacite kuti muzipewe . ( Sal . 26 : 4 , 5 ; Miy . ( Mac . 15 : 6 - 11 , 13 , 14 , 28 , 29 ) Mwacionekele , Akhristu aciyuda ndi Akhristu amitundu ina anayamikila Petulo cifukwa cofotokoza molimba mtima zimene zinacitika . Iye anakumana ndi mavuto ambili kuonjezela pa vuto la ndalama . A Inoki : Baibulo lili ndi malangizo othandiza pa mbali zonsezi . Pemphelo , kuganizila mozama pa zitsanzo za m’Baibo , ndi kuyanjana ndi anthu a Yehova , kukuthandiza anthu mamiliyoni ambili kupeza citonthozo pa mavuto awo onse . Ndinali kumutukwana ndi kumumenya . Mosiyana ndi zimenezi , iwo anali ataimvetsetsa bwino - bwino mfundo yakuti afunika kulekana na cipembedzo conama . Ndipo podzafika nthawi ya nkhondo ya dziko lonse , anali atatsala pang’ono kucokelatu m’Babulo Wamkulu . — Ŵelengani Luka 12 : 47 , 48 . Mamembala ake ni amene anakonza ciwembu cakuti aphedwe . ( Ekisodo 1 : 11 - 14 ) Farao wina anafika polamula kuti ana acimuna amene abadwa kwa Aisiraeli aziphedwa . Anacita izi pofuna kucepetsa ciŵelengelo cawo . — Ekisodo 1 : 8 - 22 . Kuphunzila Baibulo kunandithandiza kuti ndikhale wodziletsa ndi kupewa mtima wasontho . Yehova anadalitsa Yefita ndi mwana wake cifukwa ca kudzipeleka kwao , ndipo anawagwilitsila nchito popititsa patsogolo kulambila koona . Mukatelo , na imwe mudzakhala dalitso kwa anthu a Mulungu . ( b ) Kodi cozizwitsa ca ku Kana cimaonetsa kuti zinthu zidzakhala bwanji m’dziko latsopano ? Kodi tingacite motani zimenezi pamene tili mu ulaliki ? ( 2 Mbiri 20 : 5 ) Anthu amene amatsogolela pa zinthu zauzimu m’banja angatengele citsanzo ca Yehosafati . Khalani ndi maganizo oyenela Abale na alongo okondedwa amene anayamba nchito ya Yehova m’dela lathu ca m’ma 1950 , angasangalale kuona mmene coonadi capitila patsogolo . 11 : 1 - 6 ) Anthu oipa amene Solomo anagwilizana nao anamucititsa kucita zinthu mopanda nzelu moti anasiya kulambila Mulungu . Mtumwi Yakobo anafotokoza cimene cingatithandize kukhala na cimwemwe ceni - ceni na kukhala okhutila . Ngakhale n’conco , Inoki anasiyila Nowa citsanzo cabwino . Iwo anafuula kuti : “ Yehova ndiye Mulungu woona ! ” Ni makonzedwe ati olinganako amene ali pakati pa anthu a Mulungu masiku ano ? 11 : 7 , 11 . Koma m’zaka za m’ma 100 C.E , io anayamba kugwilitsila nchito mabuku ochedwa codex , cifukwa masamba ake anali kuikidwa pamodzi monga buku . 11 : 6 - 9 ) Ngakhale kuti Rudolf anazunzidwa kwa zaka zambili , koyamba ndi acipani ca Nazi , kaciŵili ndi a cipani ca Stasi ku East Germany , cikhulupililo cake sicinagwedezeke poyembekezela paradaiso padziko lapansi . Koma ofalitsa 365 m’mipingo 12 amagwilitsila nchito cinenelo cochedwa Garifuna . Amuna Anayi Okwela pa Mahosi , Na . * N’zocititsa cidwi kuti ca m’ma 1800 , ophunzila Baibulo oona mtima anayamba kufufuza ndi kuphunzila maulosi amenewa mosamala kwambili . Bruce anakamba . Mtumwi Paulo anacenjeza Akristu a ku Korinto za kuipa kolekelela anthu ocita macimo mwadala mumpingo . Kodi mwaphunzilapo ciani pa zitsanzo za acicepele athu ? Pambuyo poyelekezela , kodi muona kuti mumathela nthawi yaitali pa zinthu ziti ? ( Luka 23 : 51 ) Malinga n’zimene ena amakamba , n’kutheka kuti Yosefe kunalibe panthawi imene Yesu anali kuweluzidwa . Wophunzila Filipo anafikila ndunayo ndi kuifunsa kuti : “ Kodi mukumvetsa zimene mukuŵelengazo ? ” Kukamba zoona , zimene Yehova amaona kuti n’zamtengo wapatali n’zosiyana kwambili ndi zimene anthu amaona kuti n’zofunika . Mwacitsanzo , kumbukilani malangizo amene tinapatsidwa okhudza maphunzilo athu a Baibo . Mpingo wanu walandila kumene kalata yocokela kwa mtumwi Paulo . Kodi Satana anam’neneza ciani Yobu ? Iye anali ngati nyelele m’maso mwa Yehova , ndipo Mulungu anali wokonzeka kumuononga kothelatu . Davide anathamangila mdani wake , kwinaku akupisa m’cola kuti atenge mwala . 6 : 11 ; Hab . 1 : 2 ) Nayenso Mfumu Davide polemba Salimo 13 , anafunsa funso lofanana ndi limeneli kanayi konse . Iye anati : “ Kufikila liti ? ” ( Sal . Cigawo coyambilila pa ma voliyamu 6 , cinatulutsidwa pamsonkhano wacigawo pa August 2 , 1950 . ( Gen . 8 : 20 , 21 ; 12 : 7 , 8 ; Yobu 1 : 4 , 5 ) Koma cifukwa cokonda zinthu zakuthupi , iye anasinthanitsa mwayi umenewo na cakudya ca mphodza codya kamodzi kokha . Cokondweletsa n’cakuti m’kupita kwa nthawi , Federico anakhalanso wolimba kuuzimu , ndipo pambuyo pake anayambanso kutumikila monga mpainiya ndi mtumiki wothandiza . Iye anali kufuna mlongo woti amange naye banja , ndipo anafuna kudziŵa ngati ndingam’konde . Kuyambila m’caka cimeneco , uthengawu sukamba za Ufumu wamtsogolo , koma umakamba za boma leni - leni limene tsopano likulamulila kumwamba . Satana akatilefula zimavuta kukhalabe okhulupilika kwa Mulungu . ( Yoh . 7 , 8 . ( a ) Kodi cofunika kwambili kwa ife ndi kukhala wokhulupilika kwa ndani ? ( b ) Fotokozani mmene Paulo na Sila anathandizila woyang’anila ndende ku Filipi . Dziko la Satanali limasonkhezela anthu kukhala na mtima wofuna kuchuka na kulemekezedwa kwambili , m’malo mopeleka ulemelelo kwa Atate wathu wakumwamba , Yehova Mulungu , amene ndiye woyenela kulambilidwa na kulandila ulemelelo . — Chiv . Zoona , mapeto “ sadzacedwa . ” Tsiku limene iye anamwalila pa ngozi , linali lofanana ndi masiku onse . Ndipo m’kupita kwa nthawi , mwina makolowo adzakwanilitsa udindo umene Mulungu anawapatsa , wophunzitsa ana awo zinthu zauzimu . Koma cifukwa cabwino kwambili cokwalila m’cikwati ciyenela kukhala cakuti aŵiliwo amakondana na kulemekezana . Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zabwino zimene tikuyembekezela posacedwapa . Modziŵa kapena mosadziŵa , iwo amaonetsako mbali ya ulemelelo wa Yehova . Pa cifukwa cimeneci , munthu aliyense afunika kupatsidwa ulemu . — Sal . Mofanana ndi zimenezi anthu ambili masiku ano ali ndi “ khungu ” ponena za zinthu zimene zikucitika m’dzikoli . Atam’peza , anayamba kuonetsana ndi kuuzana mau acikondi . — Nyimbo 1 : 15 - 17 . Wofalitsa amene ali ndi cidziŵitso cocepa , adzapindulanso mwa kumuyamikila pa zimene akucita bwino ndi kum’patsa malangizo othandiza . — Mlal . Tikacita zimenezi , tidzatsatila citsanzo ca Yehova , amene nthawi zonse amaona zabwino mwa atumiki ake . [ Mau apansi ] Kodi Yosefe anatipatsa citsanzo cotani ? Monga mmene tinakambila m’nkhani yapita , ubatizo ndi cosankha cacikulu . 24 : 14 ) M’masiku ano otsiliza imeneyi ndiyo nchito yaikulu ya gulu la Mulungu . Kuonjezela apo , “ amapeleka cakudya kwa zamoyo zonse pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale . ” — Salimo 136 : 25 . N’cifukwa ciani analinganiza zakuti pacitike nchito imeneyi ? Kusintha kumeneku kukuonekelanso mu vesi 15 . Mau a mu vesi imeneyi tsopano amamveka ogwilizana bwino . Ngakhale ana anali kupempha mwaulemu tumapepa twa uthenga . Zimenezi zikuonetsa kuti mu zaka 15 zapitazi Nyumba za Ufumu zatsopano 5 pa avaleji zimamangidwa tsiku lililonse . Nthawi zina zinthu zingakhale zovuta ndipo madokotala angakuuzeni malingalilo osiyanasiyana . Motelo Yehova anaonetsa kuti amadalitsa anthu ake amene ali ndi mtima wofunitsitsa kupanga copeleka , ndipo amaonetsetsa kuti anthu akewo sakusowa ciliconse cimene cingawathandize kukwanilitsa colinga cake . ( Sal . Sara anali mkazi wabwino kwa Abulahamu , inde mnzake womuyenelela . Msonkhano wa mkati mwa mlungu umatiphunzitsa mmene tingalalikilile uthenga wabwino ndi mmene tingathandizile ena kumvetsetsa coonadi ca m’Baibulo . — Mateyu 28 : 19 , 20 . ( Aroma 15 : 16 ) Kugwila “ nchito yopatulikayi ” kumaticititsa kukhala “ anchito anzake ” a Yehova , Mulungu “ Woyela . ” ( Sal . 18 : 29 ) Pali mavuto ena amene sitingawapilile mwa mphamvu zathu zokha . Timafunika thandizo la Yehova . Gulu la nkhondo lamphamvu la Sisera linasokonezedwa . “ Sindinali kufuna kuti Akristu anzanga aziona kuti ndine munthu wabwino pamene sindinali conco . ” ​ — DANIEL Popeza tikukhala m’dongosolo lino la zinthu , tonse timavutika cifukwa ca kupanda ungwilo . Nthawi zonse , Yehova amasamalila anthu okhulupilika kwa iye . — Salimo 41 : 12 . ( Luka 19 : 1 - 9 ) Koma pamene munthu wosalungama ameneyu anamvela Yesu akuphunzitsa za Ufumu , anazindikila kuti zinthu zimene anali kumvazo zinali zofunika , ndipo sanazengeleze kucitapo kanthu . Kukamba zoona , maumboni a zakuthambo ogometsa maganizo amenewa amatithandiza kudziŵa kuti Yehova , amene “ anapanga kumwamba mwanzelu ” na dziko lapansi , afunika kum’tamanda , kum’lambila , ndi kukhala okhulupilika kwa iye . — Sal . Ife sitinadziŵe kuti abusa acipembedzo ndi amene anali ndi ulamulilo m’delalo . Abusawo anali kucititsa kuti anthu amene anali kulandila mabuku athu acotsedwe nchito . Kucita zimenezi kudzawathandiza kucita zinthu mwanzelu ngakhale pamene ali kwa okha . Nanga n’cosankha citi cimene Yehova angakondwele naco ? ’ Mmodzi wa iwo anali Monique , mlongo wa zaka za m’ma 30 wocokela ku United States . Iye anati : “ Nitabwelako ku msonkhanowo , n’napempha Yehova kuti anithandize kudziŵa zimene nifunika kucita mu umoyo wanga . Iwo anamunyadila kwambili Timoteyo . Kodi ndimanyalanyaza kupemphela ndi kuphunzila Baibulo ? ( b ) Kodi cimwemwe ca Yesu cingakhale bwanji mwa ise ? Ndiye cifukwa cake io ndi otsimikiza kuti Yehova akutsogoleladi gulu lake kudzela mwa Mfumu Yesu Kristu . Komanso , amaopseza anthu kuti amugonjele . Mau amene Yesu anakamba onena za cakudya cathu calelo ayenela kutikumbutsa zosoŵa zathu za kuuzimu . Zinthu zakale sizidzakumbukilidwanso ndipo sizidzabwelanso mumtima . ” Kodi n’ciani cingatithandize ngati tagwa ? Ca m’ma 1935 , zinaonekelatu kuti Kristu anayamba kusonkhanitsa anthu a “ nkhosa zina ” ocokela m’mitundu yosiyanasiyana . Anthu amenewa anali kudzapanga “ khamu lalikulu . ” Koma ali ku Sekemu , Yosefe anadziŵa kuti abale ake apita ku Dotana komwe kunali mtunda wa makilomita 22 kuloŵela kumphoto . 14 , 15 . ( a ) Kodi zinthu mu umoyo wathu n’zofanana bwanji na mmene zinalili mu umoyo wa Danieli ? Muzilola mzimu woyela kutsogolela maganizo na mtima wanu Kukamba zoona , Mlengi wa moyo adzaukitsadi akufa M’nkhani ino , tikambilana makhalidwe atatu amene tiyenela kupewa kuti tipambane . Ndi zinthu zina ziti zimene takhala tikugwilitsila nchito polalikila uthenga wabwino ? Anthu a Yehova ambili amayesetsa kupatula nthawi yoŵelenga Baibo tsiku lililonse , kaya ni m’maŵa , m’madzulo , kapena m’masana . Kodi n’ciani cinathandiza John ndi banja lake kupilila panthawi yovuta imeneyi ? Umenewu ndi umboni wokwanila wakuti , “ munthu amene akuyenda alibe ulamulilo woongolela mapazi ake . ” ( Yer . 1 : 9 , 10 ) Pa cifukwa cimeneci , tili na umoyo waphindu ndiponso wokhala na colinga . Mngelo wa Yehova anaona Gidiyoni akupuntha tiligu ndi mphamvu zake zonse . Yesu anaonetsa kufunika kocita zimenezi atacilitsa amuna 10 odwala matenda ofooketsa opanda mankhwala . Ndife osauka ndipo tinalibe ndalama zogulila Baibulo wina aliyense m’banja lathu . Zimenezo zinandikhumudwitsa kwambili . Koma ndinazindikila kuti tonse tifunikila Paladaiso , conco ndinapilila . Tikavula umunthu wakale , tifunika kupitiliza kupewa makhalidwe oipa amene tinali nawo poyamba . Kuceza ndi Mnzathu — Kodi Mboni za Yehova Zimakhulupilila Yesu ? Nanga mungacitenji kuti mukakambe mwamphamvu monga woimilako Mulungu wamphamvuyonse ? ( Miyambo 22 : 15 ) Tengelani citsanzo ca Yesu . Pa vesi 19 pali mwayi wosankha umene Mulungu anapatsa Aisiraeli . ( Miyambo 19 : 17 ) Iye amayamikila kwambili zimene timacitila anthu ovutika , ndipo walonjeza kukatipatsa moyo wosatha m’paradaiso padziko lapansi — ciyembekezo ca tsogolo labwino ! — Salimo 37 : 29 ; Luka 14 : 12 - 14 . N’cifukwa cake , mkulu wa nduna za panyumba ya mfumu , amene anali kuwaphunzitsa anawapatsa maina a Cibabulo . Kodi mungacite bwanji zimenezi ? ( Aroma 13 : 1 - 7 ; Tito 3 : 1 , 2 ) Apa n’zoonekelatu kuti Paulo anateteza uthenga wabwino pamaso pa akulu - akulu a boma , ndipo khoti la Kaisara inam’masula . — Afil . MAFUNSO OCOKELA KWA AŴELENGI Timoteyo sanali kudziŵa ngati adzabwelelanso kunyumba . N’cifukwa ciani Mulungu walola kuipa ? Macimo onse amene achulidwa pa Akolose 3 : 5 amagwilizana ndi kusilila kwa nsanje kumene n’kulambila mafano . Mulimonse mmene zingakhalile , tiyenela kulemekeza aliyense amene waloledwa ndi Yehova kuti azititsogolela . — 1 Akorinto 11 : 3 ; Aheberi 13 : 17 . Kumbukilani kuti mtumwi Paulo anapeleka malangizo akuti tiyenela ‘ kuyesetsa ndi mtima wonse kusunga umodzi wathu mwa mzimuwo , ndi mwamtendele monga comangila cotigwilizanitsa . ’ ( Aef . Kapena munthu wokhulupilila angagaŵane ciani ndi wosakhulupilila ? ” 20 : 28 ) Kukamba zoona , dipo ndiye inatsegula khomo kuti colinga ca Mulungu ca poyamba cikwanilitsike . ( 2 Akor . Nthawi imeneyo , Gilly , mwana wathu woyamba wamkazi anali atabadwa . Ndipo mau amene mungakhumudwe nao angakhale uphungu umene muyenela kuganizilapo . Aaron , amene amagwila nchito yokonza magalimoto , anati : “ Anthu ambili amaona kuti kugwila nchito yamanja kumawacotsela ulemu . ( Eks . ( Yoh . 6 : 19 ; 1 Ates . Pamene amake Eunice anadziŵa kuti mwana wawo wayamba kuphunzila Baibo , anauza ahedi a pa sukuluyo kuti amunyengelele kuti aleke . Koma imeneyo siinali nkhani kwa Yehova Mulungu . Kulimbikitsa ena si udindo wa akulu cabe . Timalabadila akatipatsa malamulo kapena malangizo enaake . Ndani amene safuna kukhala ndi anthu amtendele , a khalidwe loyela , ndi odalilika ? Komabe , Mulungu amaona akazi ndi amuna mofanana pamaso pake . Komabe , nthawi zina tingasemphane maganizo na Akhristu anzathu mu mpingo , ndipo zimenezi zingacititse kuti tiyambe kukwesana . Ina mwa mipukutu imeneyo inalembedwa zaka zoposa 2,000 zapitazo . Atate anamva cisoni kuona Jairo akulila . Anawapatsa zakumwa , bulasho yakuti apukutile zovala , madzi , na thaulo . “ Yehova ali pafupi ndi onse oitanila pa iye . ” — Salimo 145 : 18 Limati : “ Kuika maganizo pa zinthu za thupi kumabweletsa imfa , koma kuika maganizo pa zinthu za mzimu kumabweletsa moyo ndi mtendele . ” Conco , pangano latsopano linayamba kugwila nchito pa Pentekosite wa mu 33 C.E . , pamene ophunzila a Yesu okhulupilika anadzozedwa ndi mzimu woyela . Mapulogilamu a pa TV ndi mafilimu angaticititse kuganiza kuti kuphwanya malamulo a Mulungu pankhani ya kugonana kulibe vuto . Koma zimenezo si zoona . POKAMBA za kale lake , mlongo wina wa kum’mwela kwa Europe anati : “ Kucokela nili mwana , n’nali kuona zinthu zopanda cilungamo zokha - zokha . ” ( Luka 11 : 3 ) Koma apa Yesu sanatanthauze kuti basi tizingoganizila kuti ‘ Kaya lelo nizadya cani . ’ Conco , tizikumbukila lamulo la Yesu lakuti tiyenela kucitila anthu zimene tifuna kuti iwo aticitile . N’zoonekelatu kuti pamene Nowa ndi banja lake anatuluka m’cingalawa anayamikila Yehova kwambili cifukwa cowasamalila ndi kuwateteza . Kenako mwalephela kudikila ndipo mwacoka pamzele ndi kupita kucigayo cina . Mwacitsanzo , Mary ndi amuna ake , a David anali kutumikila Yehova pamodzi . Tuzipangizo twa mtundu umenewu tumatulutsa mahomoni m’cibalilo . ( Genesis 24 : 12 - 14 ) Kodi ndani anabwela ndi kucita ndendende zimenezo ? Iwo anasangalala kwambili pamene anadziŵa kuti dipo limatsegula mwai wopulumutsidwa ngakhale kwa anthu amene sanamvepo za Yesu . 5 : 28 ; 19 : 4 , 5 . 11 : 26 ) M’malomwake , anadalila Mulungu ndi nzelu zopezeka m’Mau ake , cifukwa zimaposa “ kukhala ndi zida zomenyela nkhondo . ” — Mlal . Kodi n’ciani cimene cimakupangitsani kulambila Mfumu yamuyaya ? Kodi lemba la Salimo 16 : 10 linakwanilitsidwa bwanji ? Kodi Yehova amateteza bwanji atumiki ake masiku ano ? A anthu ena Ngati mwamuna saonetsa cikondi ndi kuganizila mkazi wake , n’covuta kuti nkhani ya kucipinda izim’komela wamkazi . 20 : 8 ) Koma kodi Satana angasoceletse bwanji Gogi ngati iyeyo ndiye Gogi ? Iwo sanafunikenso kudela nkhawa zakuti adani awo adzawalepheletsa kutsiliza nchitoyo . Baibo imaonetsa kuti angelo ali na maina awo . ( Ower . 13 : 18 ; Dan . 12 : 1 , 13 . ( b ) Nanga n’ciani cimene analakwitsa ? Ngati mwamuna amakonda mkazi wake ndi ana , banja lake limatumikila Yehova mwacimwemwe , ndipo limakhala na mwayi wokalandila mphoto ya moyo . ( Mateyu 4 : 5 ) Luka analemba kuti Mdyelekezi “ anamutengela ku Yerusalemu , ndipo anamukweza pamwamba pa khoma la mpanda wa kacisi . ” — Luka 4 : 9 . 17 : 37 , 50 ) Zotsatilapo n’zakuti Yehova ndiye analandila citamando cifukwa ca nchito zazikulu zimenezo . N’zifukwa ziŵili ziti zinapangitsa Babulo Wamkulu kuyamba kucepa mphamvu pa anthu ? ( Ŵelengani 1 Samueli 30 : 3 , 6 . ) Kuphunzila Baibo kwam’thandizanso Delphine kusumika maganizo ake pa zam’tsogolo osati pa zakumbuyo . Buku Lapacaka yacingelezi ya mu 1929 linati : M’caka cimeneco , anthu 332 a ku Poland anaonetsa poyela kudzipeleka kwao mwa kubatizidwa . ” Mu 2013 , anafalitsa Baibulo la Dziko Latsopano lokonzedwanso . Coyamba Mfumu idzamenya nkhondo , kenako ukwati udzacitika . Rubeni asanafikebe io anacita zimene anapangana . Mpake kuti Yesu anacenjeza ophunzila ake mwamphamvu kuti akhale maso na cofufumitsa , kapena kuti ziphunzitso zimene magulu atatu amenewa anali kulimbikitsa . ( Mat . Ine sindinamveko zimenezi . Mavuto onse ali padziko lapansi , ndi umboni wakuti anthu alephelelatu kudzilamulila okha . Iwo anali anthu amene iye anawathandiza kuphunzila za Yehova , ndipo anali kuwakonda kwambili . Abale ena ali ndi luso lokamba nkhani , ndipo ena ali ndi luso locita zinthu mwadongosolo . Komanso , Yehova anapatsa Bezaleli mtima ‘ wanzelu , wozindikila , wodziŵa zinthu , kuti akhale mmisili waluso pa nchito ina iliyonse . ’ Iye ndiye “ mkate wamoyo ” weniweni . Conco , Mlengi wanzelu anapanga makonzedwe ena kupyolela mu pangano la wansembe monga Melekizedeki . 38 : 8 ; Deut . NTHAWI zonse timasangalala kukhala pamodzi pamisonkhano ndi kuphunzitsidwa ndi Yehova . Zokondweletsa n’zakuti anthu masauzande alapa ndi kuleka khalidwe lao loipa , ndipo abwezedwa mumpingo . Malinga ndi zimene Yesu anakamba , kodi uthenga wofunika umene uli m‘fanizo lake ndi wotani ? Kuganizila zimenezo kudzakucititsani kumuyamikila Yehova m’pemphelo . ( Yohane 14 : 19 ) Iye ‘ anapeleka moyo wake dipo kuwombola anthu ambili . ’ M’masiku otsiliza , anthu adzavutika cifukwa ca makhalidwe oipa ndi kusakonda zinthu zauzimu . — 2 Timoteyo 3 : 2 - 5 . Kodi Yehova anamulimbikitsa bwanji Nowa ? 10 : 4 , 5 ) Conco , tiyeni tione mmene tingagwilitsile nchito Baibulo kuti tikhalebe ndi maganizo oyenela . Ngati n’conco , kodi mungacite ciani ? Panthawiyo , mneneli Semaya anapeleka uthenga wa Mulungu kwa Rehobowamu na akalonga ake . Mlongoyo anauza mwamuna wake , amene analinso wofalitsa wosabatizika , kuti watola ndalama . ( 2 Petulo 3 : 8 ) Mwacitsanzo : Kodi ciwala cimene cimakhala cabe masiku 50 , cingamvetse mfundo yakuti anthufe timakhala zaka 70 kapena 80 ? Kukhala wolimba mtima kumatanthauza kukhala ndi cidalilo ndipo kumatithandiza kupilila mavuto . Kulimba mtima kungatithandize kuima pacilungamo . NTHAWI zambili makolo akamayang’ana ana ao akuseŵela , amacita cidwi ndi zimene anawo amacita mwacibadwa . Yehova anandionetsa kuti ndinali woyenelela kupitiliza phunzilo . ” Kukonda kwambili udindo . Zimenezi zinandisoŵetsa cocita . Anthu a m’banja langa anandiphunzitsa mmene ndingagwilitsile nchito mipeni ndi mfuti pa cocitika ciliconse cimene cinafuna kuti ndigwilitsile nchito zinthu zimenezi . ( Eks . 12 : 38 ) Pamene mlili wa 7 unacitika , ena “ pakati pa atumiki a Farao , ” anaopa mau a Yehova , ndipo anapitila pamodzi ndi mitundu yosiyanasiyana imene inatuluka mu Iguputo ndi Aisiraeli . — Eks . Koma tingaonetse bwanji kuti timam’konda ? Ngakhale n’telo , Yesu anatilimbikitsa ‘ kukhalabe maso . ’ N’zoona kuti Baibulo , zofalitsa zathu ndi misonkhano yathu zimapindulitsa anthu ambili . Mmene iye anacitila makonzedwe a Pasika kwa Aisiraeli , na mmene anakwanilitsidwila pa Yesu , zinanifika pamtima kwambili ! Mwa ici , dipo inalipilidwa kwamuyaya . ( Aheb . Musaiŵale kuti sitiyenela kudziŵa tanthauzo la mafanizo amenewa cabe , koma tiyenelanso kugwilitsila nchito zimene taphunzila m’mafanizo amenewa . Ndiye cifukwa cake kaŵilikaŵili Nyumba ya Ufumu yatsopano ikamalizidwa , anthu ambili oona mtima amene amalakalaka kudziŵa zambili za Mlengi wathu wacikondi amabwela kudzasonkhana . — Sal . Mtima woyamikila unam’sonkhezela kutumiza copeleka caufulu kuti cithandizile panchito imene anaicha kuti nchito yapadela ya Mboni . Ngati timakonda kudziona apamwamba kuposa ena , tiyenela kukumbukila kuti “ Yehova amanyansidwa ndi munthu aliyense wa mtima wonyada . ” ( Miy . Nayenso Yesu anayamba pemphelo lake la citsanzo ndi mau akuti : “ Atate wathu wakumwamba , dzina lanu liyeletsedwe . ” — Mat . Zitsulozo ziyenela kuti zinali kukhala m’mbali mwa magaleta , ndipo mwina anali kuzimangilila ku mahabu a mawilo . Apa m’pamene n’nakumana ndi asilikali aja amene nachula kuciyambi kwa nkhani . ( Luka 4 : 17 - 19 ; 24 : 44 , 45 ; Machitidwe 15 : 21 ) Ngakhale kuti anthu anali kukambanso Cigiriki ndi Cilatini panthawi imene Yesu anali padziko lapansi , Baibulo silichula ngati Yesu anali kukambanso zinenelo zimenezo . Mtsikanayo anayamba kuimba ndi kuvina mwacimwemwe cifukwa cakuti atate ake anapambana nkhondoyo . Cifukwa ca cikondi cake , Yehova amatiwongolela na kutiphunzitsa n’colinga cakuti tikhalebe mabwenzi ake , na kuti tisapatuke pa njila ya ku moyo . ( 1 Yoh . Kumatanthauza ciani kukonda Mulungu ndi ( a ) ‘ mtima wathu wonse ’ ? Mulungu , kupilitila mwa dipo , anakhululukila Paulo macimo ake ndi anthu ena a m’nthawi yake . Mu 1876 , nkhani ina imene Charles Taze Russell analemba inasindikizidwa m’magazini yochedwa Bible Examiner . Koma iye sanasiye kukhulupilila Yehova Mulungu wake . Koma iye ayenela kuti analimbikitsidwa ngako pamene Yehova anakamba mau katatu konse kucokela kumwamba oonetsa kuti anali kumudziŵa . Ndipo Akristu ena mumpingowo anayamba kuona kuti zimene munthuyo anali kucita zinalibe vuto . Buku yochedwa Cyclopedia imene McClintock na Strong analemba imati : “ Tsiku limene Khristu anabadwa silipezeka mu Cipangano Catsopano kapena kwina kulikonse . ” Nkhaniyo idzafotokoza cifukwa cake imfa ya Yesu ndi yofunika ndi mmene ingakupindulitsileni inuyo panokha . Mukamamvetsela nkhani za padziko lonse , mwina mwaona kuti zinthu zoipa nthawi zina zimacitidwa m’dzina la cipembedzo . Kodi mungapindule ndi mau odziŵika bwino akuti : ( Collins Atlas of Bird Migration ) Yehova anapatsa mbalame zokuka - kuka nzelu zacibadwa kuti zizidziŵa nthawi yokuka . Eduardo anadziŵa kuti ngati wapita kukakhalanso ndi banja lake adzasangalatsa Yehova . Ganizilani zimene iye anauza mlembi wina amene anamufunsa kuti : “ Mnzanga amene ndikuyenela kumukonda ndani kweni - kweni ? ” N’ciani cimatithandiza kupilila pa nchito yathu yolalikila ? Mdaniyo anafesa namsongole m’munda wa tiliguwo , n’kucoka . Ena amaona kuti akafika ku tuakacisi topatulika pambuyo poyenda ulendo wautali , mpamene amaonetsa kuti ndi odzipeleka pa kulambila kwao . Tinakhala nao kwa masiku aŵili kapena atatu . ( Sal . 96 : 4 - 6 ) Komabe , olambila ena a Mulungu alephela kukhala okhulupilika kwa iye ndipo acoka kumbali yake . Sitifunika kusinthanitsa miyezo yolungama ya Yehova na miyezo yathu . Cifukwa ca mfundo zimenezi , Akhristu ofika m’mamiliyoni zungulile dziko lonse aona kuti sayenela kukondwelela Khrisimasi . Ndipo Mulungu ndi anthu anapitiliza kukondwela naye . ” — LUKA 2 : 52 . Nthawi zambili anthu amafunsa Mboni za Yehova funso limeneli . Cifukwa Akanani sanali kulemekeza ngakhale kulambila Yehova Mulungu . Nanga bwanji ngati tifuna kucita maseŵela olimbitsa thupi ndi anthu ena ? Lembani zinthu zimene mufuna kuti mukacite m’Paladaiso . M’kupita kwa nthawi , anthu 5 a m’kilasi yawo anakhala Mboni za Yehova . Kupempha thandizo kwa Mkristu wokhwima mwauzimu kungatithandize kuti tisalekelele zilakolako zoipa kukula mumtima mwathu . ( Miy . Ningakonde kukatumikilako ngakhale caka cimodzi cabe . ’ Cioneka kuti Sebina atapatsiwa cilango na Yehova sanakhumudwe , koma anaonetsa kudzicepetsa mwa kulandila udindo wotsikilapo wa ukalembela . Kuti izi zitheke , tifunika kukhala ofatsa . Timaonetsa bwanji kuti timakhulupilila Yehova tikamakhululukila ena ? 14 : 12 ) Izi zionetsa kuti pali zinthu zina zimene anthufe patekha sitingakwanitse kucita . Zakeyu anali mkulu wa okhometsa msonkho , ndipo analemela kwambili cifukwa cobela anthu ndalama . Amagogomezela za kufunika kodziŵana bwino ndi munthu amene ndidzakwatilana naye . Kodi tiyenela kuiona bwanji nchito yolalikila uthenga wa Ufumu ? Kodi anthu a Mulungu masiku ano angalimbikitsidwe bwanji na masomphenya a Zekariya a magaleta ndi okwelapo ake ? Ngakhale ndi conco , mbali yaikulu ya ufumuwo munali mtendele , ndipo ophunzilawo anali kuyenda ndi kulalikila popanda zovuta . Nthawi yamtendele imeneyo inali ya zaka pafupifupi 200 . ( Aef . 5 : 26 , 27 ) Iye wavala bwino mogwilizana ndi cocitikaco . Anthu amene ali ngati nkhosa amathandiza abale a Kristu m’njila zosiyanasiyana ( Onani ndime 17 ) Buku loyambilila m’Baibulo limatiuza mmene imfa inayambila ndi mmene Paladaiso anataikila . Mwacitsanzo , akazi afunika kugonjela amuna awo , ndipo ana afunika kugonjela makolo . ( Aef . M’thandizeni kuona kuti kale - kalelo m’nthawi ya Yobu kunalibe makina oonela zinthu zakumwamba , kapena zoombo zopitila kuthambo . ( Ŵelengani 1 Timoteyo 5 : 4 , 8 , 16 . ) Yesu anacenjeza Akristu za kuonongedwa kwa Yerusalemu ndipo anasonyeza kuti zocitika za m’nthawi ya atumwi zidzafanana ndi za pa “ cisautso cacikulu . ” ( Mat . Ife timazindikila kuti munthu aliyense ali ndi ufulu wosankha zimene afuna kuti azikhulupilila . ( Oweruza 4 : 22 ; 5 : 24 ) Mungaone kuti Debora analibe nsanje . Eboo Patel amene anayambitsa bungwe lochedwa Interfaith Youth Core anati : “ Palibe cipembedzo cimene sicimaonetsa cikondi . . . , cimene sicimasamalila zacilengedwe . . . , cimene sicimathandiza anthu . ” Iye amasamalila atumiki ake okhulupilika . 1 : 28 ; 3 : 16 - 19 , 24 ) Mulimonse mmene zinalili , mfundo ni yakuti zimene Nowa anaphunzila zinamugwila mtima na kum’sonkhezela kuyamba kutumikila Mulungu . — Gen . M’pempheni kuti akuthandizeni kuyang’ana kwambili pa makhalidwe ake abwino . 5 : 1 , 2 ) . Ngakhale n’conco , Yehova anauza Mose kuti apite akalamule Farao , kuti amasule anthu a Mulungu pafupifupi 3 miliyoni amene anali mu ukapolo . Iyai , cifukwa Yehova anawalenga m’njila yakuti azimvela bwino na kukondwela pocita zinthu zimenezi . ( Sal . Iye sanatengeko mbali m’ndale kapena m’nkhondo . Iye anayamba kuyenda ndi mtumwi Paulo . Yesu anauza ophunzila ake kuti : “ Senzani goli langa . ” Kugwilizana kwake ndi kwakuti nkhani iliyonse imachula za odzozedwa a Mulungu , amene anali kutsogolela panthawi zovuta . 6 : 18 ; 1 Tim . NYIMBO : 147 , 149 Kodi mufuna kukhala ndi cikhulupililo ngati ca Davide ? Yesu anatsimikizila mau a Yehova akuti : ‘ Mwamuna adzasiya atate wake ndi amake , ndi kuphatikana ndi mkazi wake , ndipo aŵiliwo adzakhala thupi limodzi ? ’ ( Mat . Davide anakambanso kuti : “ Iye wandithandiza , moti mtima wanga ukukondwela . ” — Salimo 28 : 2 , 7 . * ( Genesis 23 : 1 , 2 ) Iye anamuyewa kwambili mkazi wake wokondedwa . Acicepele , mungapewe bwanji kukwiyila makolo anu ? Pa 2 Timoteyo 3 : 1 - 5 timaŵelenga kuti ‘ m’masiku otsiliza , ’ anthu adzakhala odzikonda , okonda ndalama , ndi okonda zosangalatsa . Motelo io anati tiyeni timuphe timuponye m’citsime copanda madzi ndipo tikanene kuti cilombo colusa camudya . Iwo tsopano anakwatiwa ndipo pamodzi ndi amuna ao akucita cifunilo ca Mulungu mu utumiki wanthawi zonse . Mwacitsanzo , pa nkhondo yaciŵili ya pa dziko lonse , anthu pafupifupi 55 miliyoni anaphedwa . Iye anati : “ Zonse zimene ndamva kwa Atate wanga ndakudziŵitsani . ” Iwo analamula Loti pamodzi na banja lake kuti atuluke m’mizindayo . ( Aheb . 11 : 39 ) Onse anali na “ ciyembekezo cotsimikizika ” cakuti Mulungu adzapeleka mbeu imene idzaphwanya Satana na kukwanilitsa colinga cake ca poyamba . ( Gen . ( 2 Akor . 4 : 3 , 4 ) Ambili a iwo akhala akuphunzitsidwa zikhulupililo zabodza na makhalidwe oipa kungoyambila ali ana . N’nali Woipa Mtima Kwambili ndi Waciwawa ( A . Anthu onse amangonileka . ( Sal . 16 : 10 ) Apa , Davide sanali kutanthauza kuti iye sadzamwalila kapena kuti sadzapita ku manda . Mu 1933 , ofalitsa anayamba kugwilitsila nchito makadi aulaliki . Cida cimeneci cinathandiza ambili kuyamba kulalikila . Mu utumiki umenewo , anawo anakhala na umoyo wabwino koposa . Mukapanga masinthidwe aang’ono , makolo angazoloŵele mwamsanga ndi kusinthako . Kumathandiza munthu kukhala pa ubwenzi wabwino na ena ndiponso kukhala na mtendele wa m’maganizo Anafufuzanso ngakhale zinthu zing’onozing’ono zimene zinali zofala panthawiyo zimene anaona kuti zikubisa coonadi . . . , kuphatikizapo ciŵelengelo ca nsomba zimene ophunzila anagwila usiku umene Mpulumutsi woukitsidwa anaonekela kwa io . Ena amakamba kuti ciŵelengelo ca nsombazo cinali 153 . ” ( Gen . 28 : 3 , 4 ) N’cifukwa cake Yakobo atakwanitsa zaka pafupi - fupi 100 , anacita zonse zotheka kuti akandile madalitso a Mulungu . 4 : 7 , 8 ; 1 Yoh . 2 : 15 - 17 ; 5 : 19 ) Kukhala pa ubwenzi wolimba na Yehova ndiye citetezo camphamvu kwa mwana kuti asasoceletsedwe na Satana , dziko lake , kapena maganizo a anthu a m’dzikoli . 12 : 1 - 3 ) Pamene Abulahamu ndi Sara anali ku Iguputo , Farao anatenga Sara ndi kupita naye kunyumba kwake kuti akhale mkazi wake . Iye sadzafa , ndipo amafuna kuti mabwenzi ake nawonso akhale na moyo wamuyaya . Komabe , Satana ndi dziko lake amafuna kutilepheletsa kukonda Mulungu . Koma zinatithandiza kudziŵa zimene zinali m’mitima yawo . ( Agal . 5 : 16 ) Mwacitsanzo , ngati ndinu mkulu mumpingo , mungapemphe mzimu woyela kuti ukuthandizeni kupeleka uphungu wa m’Malemba mwacikondi kwa ena . Mwacitsanzo , Timoteyo wa ku Lusitara anapanga zosankha mwanzelu . Zosankha zake zinamuthandiza kukhala mmishonale pamene anali ndi zaka pafupi - fupi 20 kapena kuposelapo . Mwina tingazindikile kuti tayamba kukonda zosangulutsa , anthu , zovala , ndiponso kudzikongoletsa kwa m’dzikoli . Nili na maganizo amenewo , n’navomela kuphunzila Baibo . ( Yesaya 45 : 18 ) Kukamba zoona , Mulungu ali nalo colinga dziko lapansi , ndipo monga mmene nkhani yotsatila idzafotokozela , colinga cimeneco cimagwilizana ndi ciyembekezo cokhudza tsogolo lathu . Zungulile dziko lonse , atumiki a Yehova akhoza kudzikambila okha madalitso amene alandila kwa iye . Kodi ise anthu tingatengele bwanji citsanzo cake ? Mzimu woyela unam’thandiza , ndipo nayenso anatsimikiza kuti Yesu anaukadi . Iwo anali kudzakhala osiyana ndi anthu ena cifukwa ca khalidwe lao labwino , ndi nchito yao yolalikila ‘ uthenga wabwino wa Ufumu . . . kuti ukhale umboni ku mitundu yonse . ’ ( Mat . Zimenezi zingaonekele ndi mmene mukukambila ndiponso mau amene mukugwilitsila nchito . Ndipo n’nayamba kuzonda anthu okamba Cizungu . ” “ Yehova amalanga aliyense amene iye amamukonda . ” — AHEB . ( Mlal . 12 : 1 ) Njila yokha yabwino ‘ yokumbukila ’ Yehova ndiyo kum’tumikila mokwanila . Asanabwele padziko lapansi , Mwana wa Mulungu anatumikila mokhulupilika monga “ mmisili waluso . ” Kodi buku la Levitiko limagogomezela bwanji za ulamulilo wa Yehova ? 104 : 13 - 15 ; Hag . 2 : 8 ) M’Baibo muli nkhani zambili zoonetsa mmene Yehova anasamalila anthu ake mozizwitsa . Mfumu Davide anacita cigololo ndi Batiseba . Pambuyo pake , anaphetsa Uriya , mwamuna wake . ( 2 Sam . Dziko lapansi lidzasanduka paradaiso , ndipo anthu onse okhulupilika adzakhala angwilo . Adzagwilizanitsa pamodzi mbali ya banja la Mulungu ya kumwamba ndi ya padziko lapansi . ( Chiv . Nili na umoyo waphindu ndi wokhutilitsa kwambili . ” Nzelu imeneyi idzatithandiza kuyankha mofatsa ngati wina watikalipitsa . Idzatithandizanso kukhala pa ubwenzi wathithithi na Yehova , Gwelo la nzelu zosatha . Kodi timaika bwanji coonadi ca m’Baibo m’nkhokwe yathu yosungilamo cuma cauzimu ? Timaonetsa bwanji kuti tili ndi cikhulupililo colimba ? Ngakhale kuti pa nyanja panali mphepo za mkuntho , Gust anayendetsa botiyo kwa masiku 30 mpaka kufika ku Bahamas . ( a ) Kodi mtumwi Paulo anati ciani za kulimbikitsana ? Njila imeneyi inathandiza ophunzila kuzindikila liu lake lenileni la Ciheberi , na kuphunzila cineneloco mosavuta . ( Ŵelengani Ezara 7 : 10 . ) N’kofunika kuti banja likambilane za thandizo lofunikila , mmene lingapelekedwele , ndi zimene aliyense angacite . Ine n’nali kukonda kuuka mocedwa , koma iye anali kukonda kuuka mwamsanga . Pophunzila anali kukhala pansi mopinda miyendo yake , ndipo mokweza mau anali kufotokoza zimene waphunzila . Makolo acikhristu amakondwela kwambili kuona ana awo akubatizika pamodzi ndi ophunzila ena atsopano a Khristu . ( Mac . 5 : 1 - 10 ) Mosiyana na zimenezi , cikondi ceni - ceni cimatisonkhezela kutumikila abale athu mwacimwemwe , popanda kudzionetsela kapena kufuna kuchukilapo . 6 : 27 , 28 , 31 , 34 . 18 : 1 ) Koma Davide analinso ndi anzake ena monga mneneli Natani . Mwakutelo , tidzapitilizabe ulendo wathu wa ku moyo wosatha ndi kukhala paubwenzi wolimba ndi Yehova . “ Tonsefe timapunthwa nthawi zambili . ” Conco , Yefita ataona mwana wake , “ anayamba kung’amba zovala zake ” ndi kukamba kuti mtima wake wasweka . Ndithudi , Yehova analidi kulamulila . — Gen . ( b ) N’ndani anali mtsogoleli wolonjezedwa ? BAIBO IMAPELEKA CITSOGOZO CODALILIKA KWAMBILI kwa okwatilana , makolo , komanso kwa acicepele . Ganizilani zimene zinacitikila Luigi . Waciŵili ndi wakuti , “ Aliyense wochula dzina la Yehova aleke kucita zosalungama . ” Mauthenga amenewa amawacititsa cidwi akatswili a Baibulo . Pamisonkhano imeneyi , aliyense anali ndi Baibulo ndipo anali kuliŵelenga . N’cifukwa ciani tikamba kuti lamulo la Mulungu la pa Genesis 2 : 17 silinali lopondeleza kapena losafunikila ? Yoyamba ni yakuti , pali mbali ziŵili cabe ndipo tifunika kusankhapo mbali imodzi . Anadziŵanso kuti mwana wake ndi amene anali kudzakwanilitsa malonjezo a Mulungu . — Genesis 15 : 16 ; 17 : 19 ; 24 : 2 - 4 . Mofananamo , tikamvetsetsa maganizo a Yehova ndi kuona zimene anacita m’mbuyomu , tidzadziŵanso zimene afuna kuti ticite pankhani zosiyanasiyana . Timatsogozedwa kuti tisankhe zinthu mwanzelu “ Conco ngati wina akusowa nzelu , azipempha kwa Mulungu , ndipo adzamupatsa , popeza iye amapeleka moolowa manja kwa onse ndiponso amapeleka mosatonza . ” — Yakobo 1 : 5 . Kutsatila malangizo a Petulo amenewa n’kofunikanso pa zosankha zofunika kwambili mu umoyo , monga zokhudza maphunzilo na nchito . Ndipo akhala akucita izi kucokela kale - kale . Komabe , ambili amaseŵenzetsa njila zolakwika pofuna kudzipezela ufulu . Timaona kuti n’kofunika kuthandiza ena kudziŵa dzina la Mulungu ndi kuitana pa dzinalo . Nanga bwanji alongo amene ni mbeta ? Kaini akanamvela cenjezo la Mulungu , akanapitiliza kukhala paubwenzi wabwino ndi iye . Baibo sitiuza kuti nkhaniyi inatha bwanji . Koma ubwino wake ni wakuti alongo amenewa ayenela kuti analabadila uphungu wacikondi wa mtumwi Paulo . — Afil . Anthu padziko lonse lapansi ayesetsa kuti athetse vutoli koma alephela . Izi n’zimene zinacitika kwa Naoko . Mwacionekele , Yesu anali kukamba za iye mwini , cifukwa cakuti panthawi ina iye anakamba kuti ndi mkwati . ( Luka 24 : 44 ) Motelo , pamene Akristu anali kulalikila uthenga wabwino , Ayuda ndiponso anthu osakhala Ayuda anali kudziŵa kale zinthu zina zimene Akristuwo anali kulalikila . Paulo anali kufuna kupeza anthu omwe akanamvetsela uthenga wabwino . 21 Pewani Kutenga Mbali m’Ndale za Dziko Loipali Ngakhale zinali conco , panali vuto limene linaoneka ngati sangaligonjetse . Sitingakwanitse kufotokoza zinthu zonse zosangalatsa zimene Yehova wakonzela Akhiristu odzozedwa amene adzalamulila ndi Khiristu kumwamba . ( Luka 22 : 28 - 30 ; Afil . 3 : 20 , 21 ; 1 Yoh . Iwo amadziŵa kuti angapeze cisamalilo cacikulu ngati aonetsa khalidwe labwino . Pamene Yesu anakamba za kulambila motsogoleledwa ndi mzimu , iye anatanthauza kuti olambilawo adzatsogoleledwa ndi mzimu woyela wa Mulungu . Kodi mkate umene timagwilitsila nchito pa Cikumbutso umaimila ciani ? N’zimene mayi wina ku Japan anacita . Anthu ambili safuna kuphunzitsa cikumbumtima cao . Nditapuma pa nchito , mkulu wina anandiuza kuti ndingakwanitse kucita upainiya wa nthawi zonse , ndipo anandipatsa fomu yofunsila upainiya . Koma Yehova amafuna kuti tizimvela macenjezo ake opezeka m’Baibulo kuti tizicita zinthu zabwino . Akristu oona amaonetsana “ cikondi cocokela mumtima woyela , m’cikumbumtima cabwino , ndiponso m’cikhulupililo copanda cinyengo . ” ​ — 1 TIMOTEYO 1 : 5 3 : 1 - 5 ) Komabe , munthu akadziŵa kuti mnzake wa m’cikwati anacita cigololo , koma n’kugonabe naye , mcitidwe umenewo utanthauza kum’khululukila mzake wocimwayo , ndipo umacotsapo maziko a m’Malemba a cisudzulo . ( Onani palagilafu 15 - 17 ) * Mosiyana na zolosela za anthu zimene kaŵili - kaŵili zimacokela kwa milungu yawo yabodza , maulosi a m’Baibo amacokela kwa amene analengeza kuti : “ Ine ndi amene ndimanena za mapeto kuyambila pa ciyambi . Kuyambila kalekale , ndimanena za zinthu zimene sizinacitike ” — Yesaya 46 : 10 . * Uthenga wabwino ukulalikidwa , ndipo anthu oona mtima mamiliyoni akuphunzitsidwa njila za Yehova . ( Luka 12 : 39 , 40 ) Posacedwa , Satana adzanamizanso anthu mwa kuwacititsa kuganiza kuti ali pa “ bata ndi mtendele ” m’dziko lawoli . Kulibe kwina kumene tingapeze mayankho a zoona kuposa m’Mau ouzilidwa a Mulungu , Baibo . ( Mat . 11 : 19 ) Kucotsa munthu wosalapa mumpingo ndi cinthu canzelu , ndipo kumakhala ndi mapindu ake . Mulungu anatipatsa mphatso ya Mwana wake wobadwa yekha . Imeneyi ndiye mphatso yaikulu koposa zonse imene aliyense wa ife analandila , cifukwa inatimasula ku ukapolo wa ucimo , ukalamba , na imfa . N’takhala m’kampuyo kwa miyezi 10 , asilikali otiyang’anila anaona kuti tsopano ni nthawi yakuti nivale yunifomu ya usilikali . Mtumwiyo ataticenjeza za “ kuika maganizo pa zinthu za thupi , ” anatilimbikitsanso kuti : “ Kuika maganizo pa zinthu za mzimu kumabweletsa moyo ndi mtendele . ” 6 Acinyamata ​ — Kodi Ndinu Okonzeka Kubatizidwa ? Kodi Mulungu anam’tsimikizila bwanji Eliya kuti anali wofunikabe kwa iye ? Koma popeza kuti Lazaro , bwenzi lapamtima la Yesu , anali atamwalila kale , kodi iwo anali na ciyembekezo canji ? Baibo imapeleka malangizo odalilika amene angatithandize kulimbana na mavuto athu , koma sizokhazo . Mwacitsanzo , Kalaudiyo Lusiya , mkulu wa asilikali amene anali kulamulila , anateteza Paulo amene anali Mroma . ” — Mac . 23 : 26 - 30 . Ndimacita mantha kwambili ndikakhala panja pamene palibe malo obisalako . Ponena za thandizo limene Mulungu anam’patsa , Paulo anati : “ Pa zinthu zonse , ndimapeza mphamvu kucokela kwa iye amene amandipatsa mphamvu . ” Iye sanali Mwiisiraeli , koma anamva zimene Yehova anacita kuti atulutse anthu ake mu Iguputo . Mwina muyembekezela cinthu cina cimene cingakupatseni cimwemwe , monga kutsiliza sukulu , kupeza nchito yabwino , kapena kugula motoka yanyowani . Kodi mau a Yesu atiphunzitsa ciani ? Kodi Satana ayenela kuti anali ndi colinga cotani pamene anali kuyesa Sara ? 12 : 1 - 9 ) Mwacitsanzo , Mikhail ndi Inga , anasamukila ku Russia kucokela ku Ukraine mu 2003 . Mwacionekele , mudziŵa kuti kutumikila Mulungu na mtima wonse n’kofunika kwambili . Kodi mukufuna kudzakhala ndi moyo wosatha ? Kukhala oyamikila kwandithandiza kuyamba kuona zinthu moyenela . Kuganizila yankho la funso limeneli , kudzalimbitsa cikhulupililo cathu ndi kutithandiza kukhalabe opilila . 7 , 8 . ( a ) Kodi poyamba Yehova analamula Baraki kuti acite ciani ? Kumeneko , mlongo wina dzina lake Deirdre anapitiliza kuphunzila nafe Baibulo moleza mtima . Anafunanso kum’thandiza kuti athe kulimbana ndi vuto lalikulu . N’ciani cimaonetsa kuti Yehova wakhazikitsa atumiki ake padziko lapansi ? Acibale a munthu amene amakoka fodya amakhudzidwanso . Iwo amavutika maganizo ndipo amataya ndalama . “ Inu Mulungu wathu , tikukuyamikani ndi kutamanda dzina lanu lokongola . ” — 1 MBIRI 29 : 13 . Ndinayesetsa kuleka kukoka fodya ndi kumwa mankhwala osokoneza ubongo . Kwa zaka zoposa 30 zotsatila , m’bale Brickell anayenda mtunda wa makilomita ambili - mbili kuzungulila Australia . Anali kuseŵenzetsa njinga , honda , ndiponso motoka . Ngati mudziŵa bwino kumene muyenda , cimakhala cosavuta kusankha njila yoyenelela . N’nalekanso kucita zikondwelelo za pa maholide ndi mapemphelo a kusukulu . 1 : 14 , 15 ) Satana “ sanakhazikike m’coonadi , ” koma anapandukila Yehova ndi kukhala “ tate wake wa bodza . ” — Yoh . 15 : 13 ) Kodi ise anthu opanda ungwilo tingakwanitse kutengela cikondi cimene Yehova na Yesu anationetsa ? Iye afuna kuti tisazidela nkhawa za maŵa koma tizidalila kwambili Yehova kuti adzatipatsa zimene tifunikila tsiku lililonse . 2 : 1 - 4 ) Ngati mlendo alibe wina amene akumusamalila , bwanji osamupempha kuti akhale namwe pafupi ? Lemba la Aheberi 11 : 1 ( ŵelengani ) limafotokoza bwino zimene cikhulupililo cimatanthauza . Kodi tingapewe bwanji kukumudwitsa ena mu ulaliki ? Mu 1886 , “ Msonkhano waukulu ” unakhala masiku ambili pa nyengo ya Cikumbutso . ( Miyambo 23 : 15 ) Iye sakondwela ngati tivutika , ndipo safuna kuti tife monga “ ana oyenela kulandila mkwiyo wa Mulungu , ” kutanthauza anthu osalapa . — Aefeso 2 : 2 , 3 . Conco , Yehova anawapatsa uphungu wamphamvu pankhaniyi . Tingapindule ndi ndemanga za Akristu acangu amakono , amene amakhulupilila kuti ali ndi coonadi . Mkazi wacikhiristu afunikabe kulemekeza mwamuna wake , kaya mwamunayo akucita umutu wake mwacikondi kapena ayi . — Agal . Kodi zosoŵa zauzimu za abale zinasamalidwa bwanji panthawi ya nkhondo yoyamba ya dziko lonse ? Alibe uthenga wabwino , ndiponso alibe ciyembekezo ciliconse . Koma patapita zaka ziŵili , mosayembekezela Tito anamwalila . Monga zinalili kwa otsatila a Yesu akale , timasonkhana pamodzi kuti tiphunzile na kulimbikitsana . Nadine na Didier Kaya tili mu mpingo waukulu umene uli ndi abale amene atumikila zaka zambili kapena tili m’kagulu kamene kakupita patsogolo , tiyenela kukonzekeletsa abale mautumiki amtsogolo . Tate wina wa ana 6 ku Benin ananena kuti , ngati wasankha kuti adzapenyelela DVD yophunzitsa Baibulo pa kulambila kwao kwa pabanja , iye amapelekelatu mafunso ku banja lake kukali nthawi . Iye amangotuma poganiza kuti amene adzalandila uthengawo adzacita zimenezo paokha . Masiku anonso , maso a Mulungu “ akuyendayenda padziko lonse lapansi , ” ndipo iye ndi wokonzeka ‘ kuonetsa mphamvu zake ’ kwa ife . ( Aheberi 4 : 16 ) Timaonetsanso kuti tili ndi cikhulupililo mwa Yehova pamene tim’pempha thandizo . Mofananamo , Mulungu akupeleka cenjezo cionongeko cisanafike . Mwakutelo , anapulumutsa banja lake . — Aheb . “ Ndinetu kapolo wa Yehova ! ” Matthews ) , Oct . ( b ) Ndi mafunso ati amene adzayankhidwa m’nkhani ino ? Cifukwa cakuti sitingakakamize anthu kukhala ophunzila a Khristu . Nthawi zina , tingafunike kuthandizidwa ndi ena kuti tidziŵe ngati ndifedi munthu wauzimu kapena ayi . Anayambitsa Cipembedzo ni Anthu ? 641 N’ciani cimene cingakuthandizeni kukhala ndi maganizo oyenela pankhani yokhala osiyana ndi dziko ? Makalatawo anali otidziŵitsa kuti tinaikidwa kukhala oyang’anila dela . Magulu adyela a zamalonda , amene anayelekezeledwa ndi “ amalonda oyendayenda ” pa Chivumbulutso 18 : 3 , pamodzi ndi andale ndi acipembedzo , ndiwo dziko la Satana . [ Caption on page 26 ] Anzathu : Nthawi zambili timaganiza kuti anzathu ndi anthu amene tikhala nao pafupi , kapena amene amakonda zinthu zimene timakonda . Pa cocitika cosaiŵalika cimeneco , Yesu anacita nao phunzilo la Mau a Mulungu , titelo kukamba kwake . ( b ) Ndi zinthu ziti zimene tiyenela kusamala nazo ? Cifukwa cakuti anali ndi makhalidwe abwino , anali kuyembekezela kudzakhala ndi moyo wosatha . Baibulo limatiphunzitsa kuti kudzipeleka ndi kubatizidwa ndi ciyambi ca umoyo watsopano wa Mkristu . Mfumu Solomo anachuka kwambili cifukwa ca nzelu zake monga wolamulila . Marita nayenso akanasankha kumvetsela kwa Yesu , akanayamikilidwa cifukwa cosiya zimene anali kucita kuti amvetsele kwa iye . Nkhondo yoyamba ya padziko lonse inayamba cifukwa cakuti atsogoleli a maiko sanapange zosankha mwanzelu . Lemba la Salimo 78 : 38 limati : “ Anawamvela cifundo . Pemphani citsogozo kwa Mulungu . Koma patapita cabe zaka 10 , ciŵelengelo cinawilikizika ka 10 ! Iye anauza atsogoleli Aciyuda amenewa kuti : “ Yesaya analosela moyenela za anthu onyenga inu , monga mmene Malemba amanenela kuti , ‘ Anthu awa amandilemekeza ndi milomo yokha , koma mitima yawo ili kutali ndi ine [ Yehova ] . Koma kodi umu ni mmene Yehova amaonela nchito imene timagwila pocilikiza Ufumu wake akamationa padziko lapansi ali kumwamba ? Yehova anaonetsa maganizo ake pankhaniyi pamene anadzudzula Elifazi , Bilidadi , ndi Zofari cifukwa cokamba mabodza . Mu 1987 , mwana wathu wamwamuna Yaroslav , anakukila ku Riga , m’dziko la Latvia . Kumeneko anali kulalikila momasuka . Mwacitsanzo , mlongo wacikulile angafunike kukhala wolimba mtima ngati wapemphedwa kuti akathandize mlongo wacicepele pankhani ya kavalidwe koyenela . Mumayamikila ngati wina amazindikila zimene mufuna ndi kulemekeza maganizo anu . Mofananamo , Yehova adzadalitsa acicepele onse amene amayesetsa molimba mtima kudziikila zolinga zauzimu ndi kuika Ufumu wa Mulungu patsogolo mu umoyo wawo . Koma kodi ulosi umenewu umaonetsa bwanji kuti Akristu oona anali akapolo kwa nthawi yaitali ? N’cifukwa ciani tiyenela kukhalabe maso ? ( Pelekani zitsanzo . ) ( b ) N’cifukwa ciani Satana anali kuukila Aisiraeli kaŵilikaŵili ? A Inoki : Anthu ambili amaganiza conco . Koma nkhani ya Eliya imeneyi imatikumbutsa kuti Yehova Mulungu amaona zoipa zimene zikucitika ndi kuti amacitapo kanthu panthawi yake . Cam’kangilatu Satana kufafaniza Akhiristu oona pa dziko lapansi . Iwo anakamba kuti Yehova sapindula ndi zimene timacita pom’tumikila mokhulupilika . Anakambanso kuti , kwa Mulungu , ise anthu ndise osafunika ndipo tili ngati kadziwoche , mphutsi , kapena nyongolotsi . Mau a Mulungu alinso ndi mfundo zimene zingaoneke “ zovuta kuzimvetsa , ” kuphatikizapo mbali zina zimene Paulo analemba . Ulendo wotsatila , n’napeza kuti waitana anzake ena angapo . Adresi ya ofesi ya nthambi iliyonse imapezeka pa webusaiti ya www.jw.org . Baibulo limanena kuti ‘ anamwali anzake ’ a mkwatibwi “ adzawabweletsa akusangalala ndi kukondwela . ” Pamene M’bale Harold King anali m’ndende m’dziko la China , iye analemba ndakatulo ndi nyimbo zokhudza Cikumbutso , ndipo anapanga vinyo pogwilitsila nchito tuzipatso tina tofanana ndi mphesa tochedwa black currants , ndipo anapanga mkate pogwilitsila nchito mpunga . 10 : 7 - 9 ) Pofuna kuti akapambane pa nkhondoyo , Yefita analonjeza kuti : “ Ngati mudzapelekadi ana a Amoni m’manja mwanga , ine ndidzapeleka kwa Yehova aliyense amene adzatuluka m’nyumba yanga kudzandicingamila pamene ndikubwela mwamtendele kucokela kwa ana a Amoni . ” Mtumwi Petulo anafotokoza tanthauzo la zimene zinacitikazo ndiponso cifukwa cake zinali zofunika kwambili . Kumvetsetsa mmene Yehova amatiumbila , kungatithandize kukhala paubwenzi wabwino ndi abale ndi alongo . Yesu anapeleka kwa Mulungu moyo wake wangwilo kuti abwezeletse zimene Adamu anataya ndi kuombola mbadwa zake . Tiyeni nthawi zonse tizikumbukila mau amene ali pa Miyambo 14 : 35 akuti : “ Mfumu imasangalala ndi wanchito wocita zinthu mozindikila . ” ( Machitidwe 17 : 14 ) Panthawi ina , Paulo anatuma mnyamatayo ku Tesalonika . ( Sal . 19 : 7 , 11 ; 119 : 9 , 11 ) Komanso m’Baibulo muli malangizo ndi zitsanzo zambili zimene zingatithandize kupewa zilakolako zoipa . Ine na Mairambubu tinalinso otangwanika posamalila banja lathu limene linali kukula . Panthawi imeneyo , Cilamulo ca Mose cinaletsa vikwati va pacibululu . — Levitiko 18 : 6 . Mukamapemphela , kodi mumachula mwacindunji zimene mukufuna ? 8 , 9 . ( a ) Ni mavuto ati amene othaŵa kwawo amakumana nawo m’dziko lina ? Kodi anthu a Yehova aonetsa bwanji kuti amaona nchito yolalikila kukhala yofunika ? Mulungu anakamba kuti anali monga mwamuna wa mtundu wakale umenewu . Ndipo anavutika kwambili ndi zotsatilapo zake . — Ŵelengani Miyambo 14 : 12 . “ Kukonda Mulungu kumatanthauza kusunga malamulo ake . ” — 1 Yohane 5 : 3 . N’ciani cinacititsa Petulo kuyenda pamadzi ? Nanga ife tacita zotani zofananako ? Danieli ayenela kuti anali na zaka pafupi - fupi 100 pamene mngelo wa Mulungu anamuuza kuti : ‘ Iwe Danieli , [ ndiwe ] munthu wokondedwa kwambili . ’ — Dan . ( a ) Kodi Yesu anazindikila bwanji kuti anafunika kugonjela Mulungu ? Posacedwapa , dongosolo la Satana lidzatha . Kuti tikapulumuke , tiyenela kukhala ndi cikhulupililo colimba ndi kulambila Yehova mokhulupilika pamodzi ndi gulu lake . Jimmy analeka kuwasoŵa amai ake . Mwa kucita zimenezi , Yesu anacititsa kuti zikhale zotheka kupulumutsidwa ku ucimo ndi imfa , ndiponso kudzalandila mphatso ya moyo wosatha . — Aroma 6 : 23 ; 1 Akor . Komanso , buku lina laciyuda lochedwa Wisdom of Sirach , kapena kuti Ecclesiasticus , ( 23 : 11 ) linati : “ Munthu amene amakonda kulumbila ni woipa kwambili . ” Nditaona cangu ca Apainiya apadela aŵili amene anali kutumikila pampingo pathu ndi mmene anali kuthandizila ena , ndinayamba kulakalaka kukhala mpainiya wapadela . CITSANZO COIPA CA MFUMU SAULI Ndi makhalidwe ati amene Sauli anali nao atakhala mfumu ? Pamene Timoteyo anapeza mpata wowonjezela zocita popititsa patsogolo uthenga wabwino , anaonetsa kuti anali na mtima ngati wa Yesaya , amene anati : “ Ine ndilipo ! Nanga tingaphunzile ciani kwa anthu akale monga Abulahamu ndi Mose , amene anakumana ndi mayeselo ofanana ndi athu ? Mmene munthu aliyense anakulila zimasiyana ndi ena , ndipo aliyense amakhala ndi mavuto akeake . Munthu wakhungu amatha kudziŵa zinthu m’njila zosiyanasiyana . Zotulukapo n’zakuti ngalawayo inasweka . — Machitidwe 27 : 13 - 44 . ( Maliko 15 : 41 ) Pamene thupi la Yesu linacotsedwa pa mtengo ndi kumapelekedwa kumanda , “ amai amene anayenda limodzi ndi Yesu kucokela ku Galileya , anamutsatila kukaona manda acikumbutsowo ndi mmene mtembo wakewo anauikila . KUKONDA MTENDELE Ngati umu ni mmene zinthu zilili mu umoyo wanu , mungafunike kupendanso bwino ndandanda ya zimene mumacita . Kuonjezela pa kutumikila kumalo osoŵa m’dziko la Russia , Masako anagwilanso nao nchito yokolola ku Kyrgyzstan . Anapezanso kuti ana “ amaonetsa khalidwe lopatsa , ngakhale asanayambe kukamba . Kusankha munthu wodalilika kukuimilani pankhani ya thandizo la mankhwala kudzathandiza kuti munthuyo akupangileni zosankha zoyenela ngati n’kofunika . Koma anakamba kuti tifunika kulolelana “ m’cikondi . ” Iye anati : “ Ife tili ndi udindo wolandila bwino anthu amenewa ndi kuwaceleza , kuti akhale anchito anzathu m’coonadi . ” — 3 Yoh . 8 . Kodi n’ciani cinacititsa masoka otsatizana - tsatizana amenewa ? Nanga tiyenela kukhala ndi colinga cotani pamene tiwatsatila ? Aliyense mumpingo angathandize pa mbali imeneyi mwa kulemekeza malo athu olambilila , kupeleka ndalama zothandizila kumanga Nyumba za Ufumu zatsopano , ndi kugwila nao nchito yosamalila Nyumba ya Ufumu . Mungakulitsenso cimwemwe canu mwa kukhala akhama pa nchito zokondweletsa Yehova . 35 : 11 - 14 ) Miseu yopita ku mizinda yothaŵilako anali kuilambula na kuikonza bwino . Nthawi zina , munthu anali kupelekedwa kwa Yehova monga nsembe yopseleza . Izi zinali kutanthauza kuti munthuyo adzatumikila Yehova kwa moyo wake wonse Nyengo ya Cikumbutso : ( Mat . 24 : 45 - 47 ) Ndiyeno , anapeleka mafanizo okamba za odzozedwa onse . ( Mat . Kodi io anapindula bwanji cifukwa coganizila madalitso amtsogolo ? Muzipezeka pa Cikumbutso ca imfa ya Yesu . Mothandizidwa ndi iye ndinasintha umoyo wanga mwapang’onopang’ono . Munthu wanzelu ni uja amene sacita zinthu mwaucitsilu . ” Kodi mudzakhumudwa ? Kodi mtundu waukulu ukanatuluka bwanji mwa iye ? Zitatelo anthuwo anati : ‘ Zonse zimene Yehova wanena tidzacita zomwezo ndipo tidzamumvela . ’ Akanani sanapondelezenso Aisiraeli . ( Nehemiya 8 : 8 ) Ndipo ganizilani mfundo zatsopano zimene timaphunzila mlungu uliwonse tikamakonzekela mbali ya kuŵelenga Baibulo , ndi kumva zimene ena anapindula pa kuŵelenga Baibulo kumeneko . Ofalitsa otumikila kosoŵa amenewa timawayamikila kwambili . Anali na ufulu woseŵenza , kuthandiza anthu ena , na kutumikila Yehova mwamtendele . * Ofalitsa anali kumangilila zikwangwani ziŵili , n’kuzikoloŵeka pamapewa , cina kutsogolo , cina kumbuyo . Iyi ni njila imene Mboni zinali kuseŵenzetsa poitanila anthu ku misonkhano ikulu - ikulu kuyambila mu 1936 . N’ciani cingakuthandizeni kupilila vuto limeneli ? Motelo , tili ndi cidalilo cakuti Ufumu Mulungu udzabweletsa madalitso osatha kwa anthu onse . Mu 1949 , Ella anamangidwa ndi apolisi a KGB ku Estonia . Ngati timadalila Yehova , iye adzatipatsa mzimu wake woyela kuti utithandize kucita zabwino . — Afilipi 2 : 13 . Nanga cikumbumtima cathu cingatilimbikitse bwanji kucita cabwino ? Paulo ananenanso kuti Akristu ayenela kukhutila ndi zinthu zofunikila monga cakudya , zovala ndi pogona . PITILIZANI KUYENDELA LIMODZI NDI GULU LA MULUNGU ( Luka 3 : 38 ; 1 Akorinto 15 : 45 ) Yesu ayenela kuti anali na thupi loumbika bwino , ndipo anali kulinganako na Mariya , amayi wake waciyuda . Kenako iye anaona “ mitsempha ndi mnofu zitakuta mafupawo . ” Poyankha Yesu anapeleka fanizo la Msamariya wacifundo . 3 Mbili Yanga ​ — Kukhala “ Zinthu Zonse Kwa Anthu Osiyana - siyana ” Munthu amapeza cimwemwe cokhalitsa ngati aphunzitsa ena za Mulungu ( Onani palagilafu 12 , 13 ) M’kupita kwa nthawi , zimenezi zinakhudzanso Akristu okhala ndi ciyembekezo ca padziko lapansi . Nthawi zina , anali kuyenda mzigwa za miyala ndi m’tunjila toyendamo madzi kuli kotentha kwambili uku thukuta ili paka - paka , cifukwa coyendetsa thilaki kudutsa m’mcenga wounjikana . 6 , 7 . ( a ) Kodi anthu amene apanga “ khamu lalikulu ” acokela kuti ? Angacite bwino kuganizila mmene Yehova anali kucitila zinthu ndi Aisiraeli . ( 2 Tim . 1 : 7 ) Muyenela kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ndiyenela kudzimana ciani kuti ndikwanitse kutumikila Yehova ? Kodi ena a madalitsowo ni abwanji ? Kodi kukonda Mulungu kwakuthandizani bwanji kukhala acimwemwe ? Iye analamulidwa kuti azigobola mitengo ngakhale m’nyengo yozizila . ( Mac . 10 : 22 , 24 , 34 , 35 ) Baibulo limati : “ Pamene Petulo anali kulankhula . . . , mzimu woyela unagwa pa onse [ anthu akunja ] amene anali kumvela mau amenewo . Coyamba tinafika m’zilumba za m’nyanja za Caribbean . N’cifukwa ciani kukhulupilila nyenyezi na kulosela zam’tsogolo sikungathandize munthu kudziŵa zam’tsogolo ? Baibo siikamba kuti Abulahamu anali kukhulupilila kuti akamvela lamulo la Mulungu , Isaki adzaukitsidwa pakapita maola ocepa , tsiku limodzi , kapena wiki imodzi . Kuyambila mu 1919 , misonkhano yadela ya anthu ocepa inali kucitika m’dzikoli , koma m’zaka zotsatila , ciŵelengelo ca mipingo cinayamba kucepa . Sinikayikila kuti cinali cifunilo ca Yehova Mulungu kuti izi zicitike . Sadziŵa kuti kuli boma la kumwamba la Mulungu limene Yesu Khiristu alamulila , ndi kuti posacedwa lidzapeleka ciweluzo ku maboma onse . ( Yes . Ndinaloŵanso m’kagulu ka ana a sukulu koona pa zaufulu wa ana a sukulu . 17 : 11 - 14 ) Kodi umenewu unali mwambo cabe ? Koma zinali zotheka kucotsa udindo wokhala woyamba kubadwa kucoka kwa wina kupita kwa wina . Pamene tili pafupi kuloŵa m’dziko latsopano , tiyenela kuganizila zimene Mose anauza Aisiraeli , io atatsala pang’ono kuloŵa m’Dziko Lolonjezedwa . Tingapezenso zilembo za Tetragalamatoni m’Mabaibulo ena a Cigiriki a Septuagint . Patapita zaka ziŵili , ine ndi Aarhonda , mkazi wanga wokondedwa tinamanga banja . Ndipo Mau a Mulungu amagwilizanitsa khalidwe limeneli ndi nzelu . Mu August 1954 , ndinayamba kutumikila pa Beteli ya ku Brooklyn , ndipo mpaka pano ndikutumikilabe kumeneko . Kodi n’ciani cina cimene cingakuthandizeni kuona ngati mufunadi kuyandikila Yehova ndi kum’tumikila ndi mtima wanu wonse ? Ganizilani zitsanzo izi : Cigumula cikalibe kufika , Yehova anati : “ Kwangotsala masiku 7 okha kuti ndigwetse cimvula padziko lapansi kwa masiku 40 , usana ndi usiku . ” ( Gen . 1 : 11 ) M’kupita kwa nthawi , Michiko anakwatiwa ndi m’bale wabwino , ndipo amakondwela kuti anayembekezela . Komanso , mavalidwe athu abwino adzapeleka cithunzi cabwino ca gulu lathu . ( Yakobo 1 : 17 ) Zinthu zonse zimene analenga zimasonyeza kuti ndi woolowa manja . Mulimonse mmene zingakhalile , m’malo mongopatsa anthu tumapepala , ndi bwino kuŵelenga nao Baibulo . Pa ulendo woyamba mungaŵelenge lemba limodzi kapena aŵili . ( b ) Malinga ni mau a Yesu pa Mateyu 5 : 14 - 16 , kodi tidzakambilana ciani ? Ndipo zina anakhala nazo umoyo wake wonse . Tisaiŵale kuti anamwali opusa anapempha anamwali anzelu kuti awagaŵileko mafuta . Kodi afunika kugwila nchito imeneyi pa mlingo wotani ? Nanga kufikila liti ? ( Luka 8 : 1 ) Yesu analamula otsatila ake ‘ kuphunzitsa anthu a mitundu yonse . ’ ( Mat . Anthu odzikonda amadziganizila kwambili kuposa mmene ayenela kudziganizilila . Ganizilani zimene Yehova analonjeza Davide , Mfumu ya Isiraeli wakale kupyolela mu pangano la Davide . ( b ) Kodi a “ nkhosa zina ” amawathandiza bwanji odzozedwa ? Mwa ici , anthu anali kukonda kupala moto kwa aneba awo m’malo moyatsa okha . ( Mac . 4 : 34 , 35 ) Analinso kusamalila zosoŵa zauzimu za anthu a Mulungu , ndipo anati : “ Ife tidzipeleka ndithu pa kupemphela ndi pa utumiki wokhudza mau a Mulungu . ” ( Mac . Kunena mwacidule , kumatanthauza kudzimana zinthu zina kuti tithandize ena . Ndipo ise makolo ake amatilemekeza cifukwa amadziŵa kuti tinamvela Mulungu . Makolo ambili anganene kuti nthawi imeneyo mwanayo angafunike kupatsidwa cilango . Ganizilani zimene Yesu anacita pamene ophunzila ake anatsala pang’ono kufa ndi cimphepo camkuntho . Zina mwa nkhanizo zinali kukamba mfundo mosapita m’mbali , ndipo eninyumba ena anali kukhumudwa nazo . Mungamuonetse bwanji kuti lembali linauzilidwa zoona ? Baibulo imakamba za “ mphatso yaulele ya kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu . ” ( Aef . ( Gen . Mtumwi Paulo anafotokoza cikondi cimene Yehova ndi Yesu anaonetsa kudzela m’dipo . Kale anthu a ku Iguputo anali kudya makeke ndi mikate ya mitundu yosiyanasiyana yoposa 90 . Koma wacikulile angayamikile kwambili mphatso ya coloŵa ca banja . Mwa njila imeneyo tingaone kuti ulamulilo wa Mulungu unasokonezedwa . Rudy , m’bale wokwatila wa zaka za m’ma 50 wocokela ku Netherlands , anati : “ Kutumikila kosoŵa na kuuzako coonadi anthu ambili amene sanacimveleko , kumaticititsa kukhala wokhutila . Iye anati : “ Kulalikila kumandikondweletsa kwambili . Mtumwi Paulo anakamba kuti ‘ ucimo unaloŵa m’dziko kudzela mwa munthu mmodzi , ndi imfa kudzela mwa ucimo , ndipo imfayo inafalikila kwa anthu onse cifukwa onse anacimwa . ’ — Aroma 5 : 12 . Amenewa sanali maphunzilo wamba . Iye anayelekezela kuyang’ana kwa Yehova na mmene mtumiki amayang’anila kwa mbuye wake . Nthawi zina , kulimbikitsana kungaphatikizepo kupeleka uphungu . ( Yeremiya 17 : 9 ) Conco , ngati munthu amene timakonda wacita colakwa ndipo wacotsedwa mumpingo , tiyenela kukumbukila kuti cofunika kwambili ndi kukhala wokhulupilika kwa Yehova kuposa kwa wina aliyense . — Ŵelengani Mateyu 22 : 37 . Komabe , ndinali wofunitsitsa kukambilana naye Baibulo . Iye anali wosangalala kwambili ndi zimene anali kuphunzila cakuti ndinaona monga wayamba kufuntha . Kodi nimacita bwino mbali ziti ? Ndipo anthu oposa 70 mwa anthu amenewa anayamba kutumikila Yehova , kuphatikizapo amai anga okondedwa . N’ciani cimene Yehova anacita kuti athandize anthu ? Cikondi sicicita nsanje . ” Mwamunayu anaimba Mulungu mlandu mwa kunena kuti : “ Ndimafuulila kwa inu kuti mundithandize , koma simundiyankha . Komanso , n’zodziŵikilatu kuti mpingo wanu unacita coŵinda ca ndalama zothandizila pa nchito yomanga Mabwalo a Misonkhano na Nyumba za Ufumu pa dziko lonse , kuti abale athu azisonkhanamo . Matthew anakwatila Marina ndipo Michael anakwatila Olga . Bambo anga anakukwapulani ndi zikwapu , koma ine ndidzakukwapulani ndi zikoti zaminga . ” — 2 Mbiri 10 : 6 - 14 . ( Aef . 6 : 4 ) Umenewu ni udindo wovuta , maka - maka masiku ano . ( 2 Tim . Koma kumbukilani kuti Cilamulo cimeneco cinacokela kwa Yehova . 43,034 M’kalata imene Paulo analembela abale a ku Akorinto , iye anapeleka fanizo limene lingatithandize kudziŵa mmene Yehova amaonela zofooka za anthu . Conco , Yoswa anauza ana a Isiraeli motsimikiza kuti : “ Pamau onse abwino amene Yehova Mulungu wanu ananena kwa inu , palibe ngakhale amodzi omwe sanakwanilitsidwe . ” ( Sal . 128 : 1 ; Mat . 5 : 3 ) Anatilenga mosiyana ngako na zinyama , zimene zimangokhalila kudya , kumwa , ndi kubalana basi . Paulo anati : “ Tinalimba mtima mothandizidwa ndi Mulungu wathu ndipo tinalankhula kwa inu uthenga wabwino wa Mulungu movutikila kwambili . ” ( 1 Ates . Ngati vutoli lidzayambilanso , adzakuthandiza . ’ N’cifukwa ciani kudzicepetsa n’kofunika ? Ndikudziŵa kuti Yehova adzandithandiza kuwasamalila . ” 37 : 7 - 9 . Nthawi imeneyo ndinalila , ndiyeno ndinawauza vuto langa , ndikuwapempha thandizo . Pamisonkhano , timakhala ndi mwai woonetsa kuti timakonda abale ndi alongo athu . Kodi mukhulupilila kuti mau awa adzakwanilitsidwa ? Tinapeza motoka yathu ili pa nyumba . Ndiponso tidzamvetsetsa tanthauzo leni - leni la zimene zikucitika m’dzikoli . Pamene Cikumbutso cikuyandikila , tingacite bwino kupatula nthawi yopemphela na kupenda mosamala ubwenzi wathu na Yehova . Tifunika kuŵelenga Baibulo tsiku lililonse , kusinkhasinkha pa zimene taŵelenga , ndi kupempha Yehova kuti atipatse mzimu wake woyela . Anthu anaonda kwambili ndi njala ndipo ena anali kukomoka . Iye anati : “ A bululu anga anali kunitumila ma foni ndi kuniuza kuti amayamikila kwambili utumiki umene nimacita . Kodi mumayesetsa kucita zinthu mogwilizana ndi malonjezo anu ? Ngati tikumbukila mfundo imeneyi , tidzaona cilango ca Mulungu kukhaladi umboni wa cikondi cake cacikulu pa ise . Iye anati : “ Nthawi zina zinthu zimangocitika mu umoyo , zovuta kucita nazo . YEHOVA AMATICENJEZA N’cifukwa ciani Yehova anacenjeza Kaini asanacimwe ? Mwacitsanzo , akaona kuti timaphonya misonkhano kapena cangu cathu mu ulaliki cayamba kuzilala , amatithandiza mwamsanga . 2 : 14 , 15 ) Ambili a iwo anakhala okhulupilila . Kodi kudzicepetsa kungatithandize bwanji ena akamatinyoza popanda cifukwa ? Hana anayamikila Mulungu mwa kupemphela mocokela pansi pamtima . — Ŵelengani 1 Samueli 1 : 10 , 12 , 13 , 26 , 27 ; 2 : 1 . N’naona kuti zimenezo zinali zosemphana ndi lamulo la Yesu lakuti otsatila ake safunika kutengako mbali m’zandale . 13 : 51 , 52 . Tsiku loyamba kupezeka pa misonkhano , anali ndi zaka zoposa 80 , ndipo kuyambila pamenepo sanaphonyepo misonkhano . Timayamikila kuti Yehova amatisamalila . KUTSATILA MFUNDO ZA M’BAIBULO KUMATIPINDULITSA “ Adamu womalizila anakhala mzimu wopatsa moyo . ” — 1 AKOR . Mwaphunzila ciani m’nkhani ino ? Akaganizila zocitika zimenezo Hiroo anati : Zinali zosangalatsa kwambili kuthandiza abale ndi alongo kukhala olimba mwa kuuzimu . ” Malemba Aciheberi amachula njila yofanana pa Genesis 6 : 14 . Kodi nchito imene Yehova wakupatsani ndi umboni wa ciani ? Anthu pafupifupi 8 miliyoni aphunzila coonadi ca m’Baibulo , ndipo akulalikila coonadi cimeneci padziko lonse lapansi . Acibale ndi mabwenzi ena a Mboni za Yehova anafa . Ngakhale n’conco , io anali kufuna kutonthoza anzao amene anakhudzidwa ndi ngoziyo mwa kuwauza uthenga wa m’Baibulo . Cifukwa cimodzi cakuti , angelo akugwila nafe nchitoyi . ( Yobu 1 : 9 - 11 ; 2 : 4 ; Chiv . 12 : 10 ) Ngati Yehova angatiteteze kuti tisakumane ndi mayeselo ena cifukwa coona kuti sitingawapilile , kodi sizikanaonetsa kuti zimene Satana anakamba zakuti timatumikila Mulungu cifukwa ca dyela n’zoona ? Mwacitsanzo , mayi wina amene anali wodziŵika kuti ndi wocimwa anafika kwa Yesu , ndipo anayamba kulila cakuti ananyowetsa mapazi ake ndi misozi . Cimodzi mwa zolinga za misonkhano yathu ndi kutithandiza ‘ kuganizilana kuti tilimbikitsane pa cikondi ndi nchito zabwino . ’ ( Kuti mudziŵe zambili onani bokosi lakuti “ Ubwino wa Pemphelo . ” ) ( Luka 22 : 36 , 38 ) Koma anali kufuna kuseŵenzetsa malupangawo kuti awaphunzitse mfundo yakuti safunika kucita ciwawa , ngakhale pamene ayang’anizana ndi gulu la anthu onyamula zida . Malinga ndi zimene zinanenedwelatu , anthu ndi “ odzikonda , ” osafuna kuthandiza anzao . Tingacite ciani kuti tipitilize kukonda Ufumu wa Mulungu na mtima wathu wonse ? Mosakayikila , iye adzaona kuti anacita bwino kuyembekezela moleza mtima . Ulamulilo wa Soviet Union usanathe mu 1991 , panali ofalitsa oposa 40,000 cabe . Kenako pofuna kumuyesa anamufunsa kuti : “ Kodi n’kololeka kupeleka msonkho kwa Kaisara kapena ai ? ” 1 , 2 . ( a ) Kodi Mulungu analenga ndani poyamba ? Nanga Yehova anam’gwilitsila nchito bwanji ? Mwina anaphunzitsidwa zimenezi ndi atsogoleli ao acipembedzo . Atate wathu , Yehova , watilonjeza kuti adzatipatsa zinthu zimene tifunikiladi ngati tiika Ufumu ndi cilungamo cake patsogolo . ( Mat . Federico 3 : 20 ) Mulungu anapatsa anthu aŵili oyamba mphatso yamtengo wapatali . Mose anadziŵa zimenezi , ndipo anacita zonse zimene Yehova anam’lamulila . Anthu anali kukonda kumvetsela zokamba za Yesu cifukwa cakuti anali kulankhula ‘ mogwila mtima , ’ ndi mokoma mtima . Komabe , zinthu zimenezi siziyenela kutibweza m’mbuyo . Yehova amatitsimikizila kupyolela m’malemba kuti adzakhala ndi anthu amene ‘ akuyenda m’cigwa ca mdima wandiweyani . ’ ( Sal . Mwaŵelenga bwino . “ Kugwila nchito mwamphamvu n’kosangalatsa . Panthawiyo , munthu wina anabyala namsongole m’munda wa mnzake cakuti zonse zimene mwinimunda anabyala zinawonongeka . 12 : 7 - 9 ) Conco n’zomveka kunena kuti pa nkhondo ya Armagedo , magulu a nkhondo a Kristu ndi angelo oyela . Kuti mucite zimenezi muyenela kuipemphelela nkhaniyi ndi kuiganizila mwakuya . Dzinali limatanthauza kuti , “ woweluza wanga ni Mulungu . ” ( Dan . Malemba amalimbikitsa tonse kupita patsogolo . ( 1 Tim . ( 2 Petulo 3 : 9 ) Conco , Mulungu asanawononge anthu oipa , tiyeni tipitilize kulengeza uthenga wocenjeza anthu kuti ambili akapulumuke . Ndimapitabe ku masitolo akuluakulu osati kukacitila anthu zacinyengo , koma kukawauza za cikhulupililo canga . Jim anati : “ Aliyense anathandiza kuti zinthu ziyende bwino . ” Ndipo nditafufuzanso za caka cimeneci ca 1914 m’bukuli limene timagwilitsila nchito pophunzila Baibulo , ndinapezamo mfundo zoonjezeleka . Baibo imatiuza kuti : “ Pali kumwamba kwatsopano ndi dziko lapansi latsopano zimene ife tikuyembekezela mogwilizana ndi lonjezo lake , ndipo mmenemo mudzakhala cilungamo . ” ( 2 Pet . Wamasalimo anati : “ Zolinga za Yehova zidzakhalapo mpaka kalekale . Maganizo a mumtima mwake adzakhalapo ku mibadwomibadwo . ” Amayi anali atapezako zofalitsa zophunzilila Baibo , ndipo n’nali kukonda kuziŵelenga , makamaka kuonamo mapikica . Panthawiyo mu Tuvalu munali ofalitsa obatizidwa atatu cabe . Kodi pali ciyembekezo canji cokhudza tsogolo lathu ? Usiku , civomezi camphamvu cinagwedeza maziko a ndendeyo cakuti zitseko zonse zinatsekuka . Maseŵela a baseball ananibweletsela ulemelelo na ndalama , koma zinthu zimenezi sizinakhalitse . Komanso , n’nadziŵa kuti siningakhale pa ubwenzi na ena ngati ine sindili pa ubwenzi na Yehova . Onetsetsani kuti pamalopo palibe congo . Mwana wathu woyamba wamkazi Irina , ndi banja lake , amakhala ku Germany . Tsiku lina titauka m’maŵa , tinapeza kuti zofunda zathu zauma ku mbali ya kumutu , ndipo zinali mbuu cifukwa ca nthunzi zathu . 22 : 37 - 39 ) Tikakhala wolimba mtima , sitidzaleka kulalikila . Kuganizila citsanzo ca Yesu kumathandiza munthu kukhala mwamuna ndiponso tate wabwino MFUNDO YA M’BAIBO : ‘ Nikhulupilila kuti ucita zimenezi . Ndikudziwa kuti ucita ngakhale zoposa zimene ndanenazi . ’ — Filimoni 21 . Satana amayesetsa kuti atikope ndi zinthu za m’dzikoli , ndiponso kuti atisokoneze potumikila Yehova . Ndipo kusintha kwa zinthu , kukhoza kuwonjezela kapena kucepetsa utumiki wanu . Ngakhale acicepele anali kufuna kukhala pafupi na Yesu , cifukwa Baibo imati : “ Anatenga anawo m’manja mwake . ” — Maliko 10 : 13 - 16 . ( 1 Ates . 5 : 21 ) Tikatelo , tidzapambana polimbana ndi Satana , dziko lake , ndi zizoloŵezi zoipa . Conco , ndinapemphela kwa Yehova ndi kusinkhasinkha zimene Baibulo limakamba ponena za cikondi cake . Ayuda anaukila ulamulilo wa Aroma , ndipo mu 66 C.E . asilikali a Roma anatsala pang’ono kuononga mzindawo . Yesu Khiristu nayenso anadalitsidwa cifukwa cokhalabe womvela Mulungu pokumana ndi mayeselo osiyana - siyana . Mzimu wake woyela udzatithandiza kumvela malangizo onse amene akulu amatipatsa . Kwa miyezi itatu , tinali kukambilana Baibulo mwa apa ndi apo , ndipo makambilano athu anali kufika mpaka usiku . Fotokozani citsanzo ca mmene tate wacikondi anatetezela mwana wake . Nanga mungapindule bwanji ? ( Akol . 3 : 12 ) Iwo amagwilizananso kwambili akalola ‘ mtendele wa Kristu kulamulila m’mitima yao . ’ Koma limati adzakhala okonda zosangalatsa ‘ m’malo mokonda Mulungu . ’ ( Miyambo 4 : 3 ; Tito 2 : 4 ) Samuel , amene amakhala ku Australia , anakamba kuti : “ Pamene ndinali wamng’ono , Atate anali kundiŵelengela Buku Langa la Nkhani za M’baibo usiku uliwonse . Ambili amene sakwanitsa kufika pamisonkhano amasangalala kumvetsela misonkhano pa foni . Pamene Yesu anafunsa Petulo kuti : “ Kodi umandikonda ine kuposa izi ? ” Komabe , ngakhale masiku ano , zimene zinacitika m’nthawi ya Mose ndi m’nthawi ya Akristu oyambilila zingacitikenso . Iye akufuna kuti io alalikile uthenga wabwino padziko lonse , ndipo sadzalola ciliconse kusokoneza nchitoyi . Iye wathandiza anthu ake kumulambila m’njila imene amaivomeleza mwa kuwalekanitsa ndi cipembedzo cabodza . Kenako anandifunsa kuti : “ Iwe , likulu la Mboni za Yehova lingakhale bwanji m’Baibulo osati ku America ? ” 11 : 28 - 30 ; 1 Akor . ( Ŵelengani Luka 22 : 27 . ) Posapita nthawi , amayamba kupeza njila zoti akumane . Tiyenela kukumbukila kuti cilakolako coipa cingapangitse kuti ticite chimo . ( b ) Tifunika kucita ciani kuti tikatetezedwe ndi Yehova ? Anthu amene anapulumuka m’nthawi ya Ezekieli sanaikidwe cizindikilo ceniceni pamphumi zawo . Patapita nthawi yocepa kucokela pamene Yesu anaphedwa , mpingo wonse wacikhiristu unaloŵa m’nyengo yamtendele . Koma Timoteyo sanali conco . A Daka : Tsiku lina ndinali kukamba ndi mnzanga wa kunchito . Komabe , zioneka kuti Yesu anali kukamba za ciukililo ca kumwamba . Mkaidi wina amene anali pulofesa wa masamu anacita cidwi ataona khalidwe lathu labwino , ndipo anatifunsa mafunso okhudza zikhulupililo zathu . A hedi a pa sukulu pathu , amene anali m’busa wa Anglican , ananicotsa sukulu . ( Mat . 6 : 21 ) Conco , kukonda Yesu na mtima wonse , kudzatilimbikitsa kuganiza , kukamba , na kucita zinthu zoonetsa kuti timaika zinthu za Ufumu patsogolo osati zakuthupi . — Afil . ( b ) Tidziŵa bwanji kuti kukhala m’jele sikungalepheletse munthu kukhala na ufulu umene Yehova amapeleka ? Iye anapemphela kwa Yehova ndi kumuuza nkhawa zake . Ndiyeno , analemba makalata ku maofesi a nthambi ambili kuti adziŵe mavuto amene alongo osakwatiwa angakumane nao . Zingakhale zomvetsa cisoni ngati tingasinthe maganizo athu pankhani yokhudza kudzipeleka kwa Yehova , cifukwa zimenezi zingapangitse kuti tidzaonongedwe . Davide anakhumudwa kwambili cifukwa ca kusakhulupilika kwa mwana wake komanso anthu ena amene anali kuwadalila . Baibo imapeleka yankho pamene imati anthu analengedwa “ m’cifanizilo ca Mulungu . ” Izi zitanthauza kuti anthu ali ndi makhalidwe amene Mulungu ali nawo . — Genesis 1 : 27 . Kufunsila nzelu kwa anthu amenewa kungakhale kothandiza , koma muyenela kukhala wosamala . Zimene Mulungu Adzacita Pothetsa Zinthu Zoipa 7 5 : 20 ) Akhristu oona amayesetsa kupewa makhalidwe amenewa . Pambuyo polalikila maulendo angapo ku Balykchy , tinazindikila kuti m’tauniyo munali anthu ambili acidwi . Ŵelengani Mateyu 13 : 31 , 32 . N’zimene wacicepele wina , dzina lake Luca anacita . ( Yes . 41 : 8 , 9 ; 49 : 8 ) Masiku ano , Yehova amakomelanso mtima anthu amene amalapa moona mtima . — Sal . kufunika koyang’anitsitsa pamphoto yathu ? Musalole kuti zimenezi zikucitikileni ngakhale pang’ono . ” Popeza tili ndi zikhalidwe zosiyanasiyana , tiyenela kudziŵa zimene tingacite kuti Yehova apitilize kukhala “ Mulungu wathu . ” Koma cifukwa cakuti anali wofunitsitsa kukamba nkhaniyo , anakamba nkhani yonse uku akulila . ” Kodi ndikambilane naye za nkhaniyi ? ’ MASIKU ano , timakumana na mavuto oculuka . 3 : 15 . Ine ndikhala wokuposa pa ufumu wokha . ” — Genesis 41 : 38 - 41 . 21 Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi 116 : 1 ; 136 : 24 - 26 . Mafunso amene omasulila anali kufunsa anaonetsanso kuti mau ena a m’Baibulo angathe kumveka molakwika . Kristu wakwela pa hachi ‘ cifukwanso ca cilungamo . ’ Cikondi ceniceni cimatisonkhezela kutsatila malangizo a m’Baibulo akuti : “ Aliyense asamangodzifunila zopindulitsa iye yekha basi , koma zopindulitsanso wina . ” — 1 Akorinto 10 : 24 . ( Mac . 21 : 17 - 20 ) Koma Paulo anawaongolela ndi kuwathandiza kumvetsa mfundo yakuti macimo ao anakhululukidwa cifukwa ca nsembe ya Yesu osati nsembe ya nyama . ( Aheb . 10 : 5 - 10 ) Ambili mwa Akristu amenewo analandila malangizo a Paulo ndi kusintha maganizo ao . M’nkhani yoyamba , tidzakambilana mmene Yehova wakhala akutsogolela anthu ake kuphunzila zinthu pang’onopang’ono m’njila yosavuta ndi yomveka bwino . Koposa zonse , zikanakhala kuti Mulungu sanacitepo kanthu pa ucimo wa mu Edeni , kukhulupilika kwake kukanakhala kokaikitsa . Monga mmene Akhiristu aciheberi anacitila , ifenso tingaŵelenge ndi kucita zinthu mogwilizana na colinga ca Mulungu cimeneci . Potumikila monga woyang’anila msonkhano wacigawo , n’naona kuti m’bale Franz analidi wofunitsitsa kucita zinthu poganizila cikhalidwe ca anthu . Kuwonjezela apo , Mulungu sacita zinthu cifukwa ca mkwiyo , ngati mmene anthu ambili amacitila . Sitidzacita kupempha ena kuti atiuze zocita . Fotokozani nkhani ya m’Baibulo imene ionetsa maganizo odzinama amene anthu ena a Yehova anakhala nao . Ndipo palibe mphatso imene inakwanilitsapo cosoŵa cathu cacikulu kuposa nsembe imene inatimasula ku ucimo ndi imfa . Conco , tili na cikhulupililo cakuti mwa Mau a Yehova , mzimu wake , na khama lanu , mudzakwanitsa kuthandiza ana anu kukhala na ‘ nzelu zowathandiza kuti akapulumuke . ’ Mfundo zimenezi sizilola Akhristu kukhala na mfuti ya mtundu uliwonse kuti adziteteze kwa anthu anzawo . Cinanso , pamene tifuna kuŵelengela munthu lemba , tifunika kukamba mau amene angamuthandize kulemekeza Baibo . 3 : 8 , 9 . 1 , 2 . ( a ) Kodi Mose anapanga cosankha cotani ali ndi zaka 40 ? Sipadzakhalanso kulila , kapena kubuula , ngakhale kupweteka . Zakalezo zapita . ” — Chivumbulutso 21 : 3 , 4 . Zaka zambili zapitapo , ndipo tonse aŵili tili ndi zaka za m’ma 80 . Nkhaniyi itilimbikitsa kuti tipitilize kupezeka pamisonkhano . ( a ) Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti ndi wodzicepetsa ? NYIMBO : 88 , 41 Ndipo mudzakhala wokondwela paumoyo wanu wonse . Sindifuna kumva ciliconse cokhudza cipembedzo canu . 17 , 18 . ( a ) Fotokozani mwacidule mapangano 6 amene takambilana amene amagwilizana ndi Ufumu . ( b ) N’cifukwa ciani tiyenela kukhala ndi cikhulupililo cosagwedela mu Ufumu ? Baibo ni mau ouzilidwa na Mulungu Wamphamvuyonse amene analembedwa kuti akuthandizeni . * Kuti tikhale mbali ya banja la Yehova , tiyenela kukhala aukhondo kapena kuti oyela . ( Ŵelengani Mateyu 12 : 39 , 40 ) Yesu anakamba kuti nthawi imene Yona anali m’mimba mwa nsomba , inali kuimila nthawi imene Yesu adzakhala m’manda . Akristu a m’nthawi ya atumwi naonso anali kucita zinthu mogwilizana . Kodi mau akuti “ maufumu a anthu ” mwawaona ? N’cifukwa ciani tiyenela kudzipenda nthawi zonse ? Koma kunamupatsa mwayi wopeza mabwenzi ena atsopano , amene mosakayikila adzakhala anzake kwa moyo wake wonse . Ufulu womasuka ku ciani ? Mwacionekele , ngakhale Hezekiya , sanali kuyembekezela zimenezo ! — 2 Maf . Mofananamo , cikondi ca abale ndi alongo athu cingakuthandizeni kukhala Mkristu wofikapo . ( Mac . 6 : 1 - 6 ) M’kupita kwa nthawi , abale enanso anaikidwa m’bungwe lolamulila . ( Mac . Lomba tiyeni tikambilane njila ziŵili za mmene tingawathandizile . Yelekezani kuti mukuona mkazi wa ku Middle East , wa maso okongola mocititsa kaso . Pamene anali padziko lapansi , Yesu anacilitsa anthu odwala matenda monga khate ndi khunyu . N’zocititsa cidwi kuona kuti olemba Malemba Acikristu Acigiriki akagwila mau m’Malemba Aciheberi , nthawi zambili anali kugwila mauwo kucokela m’Baibulo la Septuagint . Ngakhale kuti anali kudziŵa kuti Yesu anagwilitsila nchito vinyo pa Cakudya ca Madzulo ca Ambuye , magazini ya Watch Tower inali kulimbikitsa kugwilitsila nchito juwisi weniweni wopangidwa kucokela ku mphesa zongokolola kumene kapena zouma , poopela kuti amene ali ndi “ cifooko cakumwa mowa ” asaikidwe pa ciyeso . M’dziko limenelo “ mudzakhala cilungamo ” ndipo cinyengo sicidzakhalamonso . — 2 Petulo 3 : 13 . ( 2 Akorinto 9 : 7 ) Caka catha , Mboni za Yehova zinalalikila uthenga wabwino kwa maola pafupifupi 2 biliyoni ndipo zinali kucititsa maphunzilo oposa 9 miliyoni mwezi uliwonse . Pamene dzikoli likutitimila m’makhalidwe oipa , tifunika kudana ndi zoipa , monga mmene Yehova amazizondela . ( Sal . Lembali linan’thandiza kuganizila amene amabweletsa mayeselo amenewa . Pa avaleji , munthu mmodzi amafa m’masekondi 6 alionse . Cimayembekezela zinthu zonse , cimapilila zinthu zonse . 5 : 8 ) Nayenso Petulo analemba kuti : “ Ngakhale kuti simunamuonepo [ Yesu ] , mumamukonda . Pa ulendo wina , apainiya anzanga ananipelekeza ndipo tinayendela m’motoka yanga . Koma ndamva kuti iweyo ukamva maloto umatha kumasulila . ’ ” Koma bwanji ngati tayamba kuika maganizo athu onse pa zofuna zathu ? 133 : 1 ) Amasangalalanso kukhala m’gulu la abale a padziko lonse , amakhala na umoyo wabwino , komanso amakhala na ciyembekezo cabwino ca m’tsogolo . Baibulo limatiuza kuti Yesu asanakhale munthu , anali pambali pa Mulungu kumwamba “ monga mmisili waluso . ” — Miy . N’navutika maganizo kwa mawiki angapo . Munthu angandicite ciani ? ’ ” 7 , 8 . ( a ) Abulahamu ndi Sara anakumana ndi mavuto otani ? Amatimvetsela , kutilimbikitsa , na kutipatsa uphungu woyenela wa m’Malemba . ( b ) Ni kusiyana kwanji pakati pa anthu kumene Yehova amaona akayang’ana pa dzikoli ? M’malo mwake , kungacititse cabe munthu kumwalila msanga . Mosakaikila , Yesu anali kusamalila ndevu zake na kuzidulila bwino . Anali kudulilanso bwino tsitsi lake . ( Mateyu 24 : 14 ) Mapeto amenewa amachedwanso “ tsiku lalikulu la Mulungu ” kapena kuti “ Haramagedo . ” Conco , anatiphunzitsa kuyendetsa , cakuti pambuyo pake tinali okonzeka kuyenda ulendo wathu . 23 : 6 , 7 . Pamene n’nafika , n’napezekapo pa msonkhano wakuti Dziko Latsopano wa mu 1953 . Maulendo amenewa anatipatsa mwayi woyamikila zimene acicepele ndi acikulile amacita potumikila mokhulupilika , komanso kuwalimbikitsa kuti apilitize kutumikila Yehova mu utumiki wawo wa mtengo wapatali . Tinali okwanila 6,000 ndipo tinaimilila m’munda wamatope kuti timvetsele nkhani yolimbikitsa imene M’bale Knorr anakamba ya mutu wakuti : “ Wolamulila Wosatha wa Mitundu ya Anthu . ” Umoyo Wanga Unali Kuipilaipilabe 10 Zimenezi zimalimbikitsa mgwilizano ndi ubwenzi . ▪ Kukonzekeletsa Anthu ‘ Kuphunzila Zokhudza Yehova ’ Iye anali kudziŵa zinthu zimene zinali zofunika kwambili . Mukudalila Yehova kwambili , ndipo simukaikila kuti adzakwanilitsanso zinthu zina zimene walonjeza . Inati : “ Kucimwila lamulo la Mulungu kumaticititsa kukhala ndi nkhongole kwa iye . . . . 16 : 25 ) Mitima ndi maganizo awo zinakhala mmalo cifukwa ca mtendele wa Mulungu . 34 : 7 ) M’malomwake , tifunika kukhala otsimikiza kuti atumiki a Mulungu padziko lonse adzapitiliza kupita patsogolo mwauzimu . Mosakayikila ! Nanga mwacikondi tingalimbikitse bwanji ena kupanga zosankha zoyenela pankhaniyi ? Tifunika kupilila mpaka pa mapeto , osati cabe kwa kanthawi . Nikavalila sukulu , n’nali kuyenda nawo muulaliki . Mwacionekele , ulosiwu sunali kudzakwanilitsidwa pa Nebukadinezara cabe , koma unali kudzakwanilitsa mbali ina yofunika kwambili . ( Aroma 5 : 6 - 8 ) Mtumwi Yohane analemba kuti : “ Mulungu anatisonyeza ife cikondi cake pakuti anatumiza m’dziko Mwana wake wobadwa yekha kuti tipeze moyo kudzela mwa iye . N’cifukwa ciani Yosefe anafunika kukhala woleza mtima ? Yesu nayenso n’citsanzo cabwino pankhani ya kuonetsa cifundo . Kuti timvetsetse tanthauzo la kutumikila Mulungu ndi mtima wathunthu , tiyeni tikambilane za Asa ndi mafumu ena aciyuda , amene anatumikila Mulungu ndi mtima wonse . Iye pamodzi ndi mnzake Elisa anapitiliza kulengeza uthenga wa Mulungu ndi kupilila zinthu zopanda cilungamo . Koma n’tayamba kuphunzila Baibo , n’nazindikila kuti nifunika kuyamba ndine kusintha mtima wanga . Monga Alex amene tamuchula pamwambapa , anthu ambili safuna kugwila nchito yolemetsa . Kodi tidzasunga mkwiyo kwa nthawi yaitali na kuulekelela kukula ? ( b ) N’zinthu ziti zimene tingacite kuti tithandize ofooka ? Wafuntha naco cipembedzo ! ” Patapita miyezi 9 , tinamanga banja pa 30 January , 1954 . Mwacitsanzo , ganizilani zimene zinacitika Abulahamu atangouzidwa kuti adzakhala “ mtundu waukulu . ” ( Gen . Wolemba Uthenga Wabwino , Maliko , anati : “ Yesu anapita ku Galileya kukalalikila uthenga wabwino wa Mulungu kuti : ‘ Nthawi yoikidwilatu yakwanilitsidwa ! Ufumu wa Mulungu wayandikila ! Lapani anthu inu ! Pitani polemba kuti MABUKU > MABUKU NDI TUMABUKU . Pokamba za atumiki okhulupilika a Mulungu , Baibo imati : “ Pita ukadye cakudya cako mokondwela ndi kumwa vinyo wako ndi mtima wosangalala . ” — Mlal . ( Mac . 4 : 13 ) Atsogoleli a cipembedzo aciyuda anaphunzila miyambo yacipembedzo ku masukulu ophunzitsa zacipembedzo , koma ophunzilawo sanaphunzile zimenezo . Koma tinalinso ndi m’bale wacikulile Eldon Woodworth , amene anali wodzozedwa . Mukatelo , mudzayamba kum’dalila kwambili . Yehova anawapulumutsa . Tiyenela kumukonda na kudzipatulila kwa iye . — Ŵelengani 1 Akorinto 8 : 3 . Pambuyo pake , anadzipeleka kukagwila nawo nchito yomanga likulu latsopano ku Warwick , mumzinda wa New York . ( Mat . 22 : 37 - 39 ) Koma Malemba amene ali m’palagilafu yapitayi , ationetsa kuopsa kotsatila mtima wathu pocita zinthu . 15 : 25 ) N’zoona kuti nthawi yoyembekezela ndi yaitali kwambili , koma kuyembekezelako kudzakhala kwa phindu . Zili conco cifukwa ngati timakhululukila ena monga mmene Yesu anatiphunzitsila , timateteza na kulimbitsa mgwilizano wathu wamtengo wapatali . Iye anati : “ Cifukwa n’nali kuifunitsitsa ngako . ” Baibo imacha mfumu imeneyo kuti “ Mfumu yamuyaya . ” ( 1 Tim . Koma panapita zaka 14 kuti mau a Mulungu akwanilitsike . — Gen . Mwacitsanzo , ganizilani mmene Mulungu anathandizila mwana wake kupoletsa matenda amene madokota analephela kucilitsa . ( Mat . Iye anakamba za kukula kodabwitsa kwa kanjele ka mpilu poonetsa mphamvu imene Ufumu wa Mulungu uli nayo yokulitsa , kuteteza ndi kugonjetsa mavuto onse . Lembali likuonetsa kucepekela kwa cakudya cakuti kilogalamu imodzi ya tiligu ingagulidwe ndi dinali imodzi , imene inali malipilo a tsiku lathunthu m’zaka 100 zoyambilila . M’mipingo 309 ya ku Panama , muli apainiya apadela oposa 180 . ( Miyambo 3 : 21 ) Iye anati : “ Ngakhale kuti ndinali kugwila nchito ku kampani ya zamagetsi , ndinali kugwilanso nchito iliyonse imene ndapeza , kuti ndipezeko ndalama . Iye anaona zimene Gidiyoni akanatha kucita , ndipo anadziŵa kuti adzam’gwilitsila nchito kulanditsa Aisiraeli . — Ŵelengani Oweruza 6 : 11 - 16 . 6 : 9 , 10 ) Komabe , kungotsatila miyezo ya Yehova ya makhalidwe abwino si kokwanila . ( Miy . 12 : 25 ) Ngati muululila wina nkhawa zanu mosabisa kanthu angakuthandizeni kumvetsa zinthu ndi kudziŵa mmene mungacitile nazo . Tinatumila foni m’bale wina amene anabwela ndi kutipeleka ku nyumba kwake na kumisonkhano ya mpingo . Ngakhale ndi telo , ndi anthu ocepa cabe amene anali kumvetsetsa tanthauzo la mau a Yesu . Ena amauka m’maŵa kuti aŵelenge , kusinkhasinkha , ndi kupemphela . Yehova ndi Mulungu wa Dongosolo , 5 / 1 5 : 27 - 29 ) Pofuna kutithandiza kuti tipitilize kukonda Ufumu wa Mulungu na mtima wathu wonse , Yehova watipatsa cinthu cina cimenenso ni cuma camtengo wapatali . ( Aroma 8 : 23 ) Zoona , ciyembekezo cawo n’cokakhala ana a Mulungu kumwamba . Ndinaphunzila Cilatini , ndi za umoyo wa “ oyela mtima ” a Cikatolika , ndiponso ndinali kulambila Mariya . Ponena za mwamuna wake , mkazi wina wa ku Spain wochedwa Rosa anakamba kuti mwamuna wake “ anali munthu wabwino kwa anthu ena , koma kunyumba anali munthu wankhanza . ” Yobu anapewelatu kulambila mafano kwa mtundu uliwonse , ngakhale kwa mumtima cabe . Koma anacitanso zambili . Kuti ndipeze malo ogona ndinali kuphwanya galimoto za anthu ndi kugonamo mpaka m’bandakuca . Zaka 2,000 zapitazo , Baibo inakambilatu kuti , “ nthawi yapadela komanso yovuta , ” idzakhala ‘ m’masiku otsiliza . ’ N’cifukwa ciani tiyenela kumuyamikila Yehova nthawi zonse ? Ngati atate kapena amai anu akudwala matenda osacilitsika , ndi bwino kudziŵa zoloŵetsedwamo . M’nkhani ziŵilizi , tidzakambilana zitsanzo za m’Baibulo zimene zingatithandize pankhaniyi . * Kamakamba kuti nidzaonananso na mnzangayo m’Paradaiso . Mulungu anafuna kuti Kaini amvele cenjezo ndi kuti ‘ amuyanje . ’ Iwo anandiphunzitsadi . Yesu ndiye Mtsogoleli wathu , ndipo Baibulo limatilangiza kuti tiyenela kutsatila iye yekha cabe . — Mateyu 23 : 10 . ( c ) Nanga cimakhudza bwanji utumiki wathu ? Yendani pa webusaiti ya jw.org , imene ipezeka m’vitundu voposa 900 . Mudziŵeni bwino Wopeleka mphatso . Conco anacondelela Yehova kuti amuthandize kuthetsa vutoli ndi kuonjezela utumiki wake kuti ayenelele kukhala mpainiya wa nthawi zonse . Zaka zambilimbili zimenezi zisanacitike , Ezekieli nayenso anatengedwela ku kacisi m’masomphenya . — Ezekieli 8 : 3 , 7 - 10 ; 11 : 1 , 24 ; 37 : 1 , 2 . Baibulo linakambilatu za nyengo imene anthu ‘ adzaononga dziko lapansi . ’ Makolo afunika kudziŵa bwino zimene ana awo amafunikila . Musandisiye pa nthawi imene mphamvu zanga zikutha . ” M’bale Mark Sanderson , amenenso ali m’Bungwe Lolamulila , ndi amene anakamba nkhani ya malilo a M’bale Pierce , ku Beteli ya ku Brooklyn pa Ciŵelu , pa March 22 , 2014 . Iyai , anali kudziŵa , n’cifukwa cake Malemba amati “ Adamu sananyengedwe . ” ( 1 Tim . Amenewa ndi Ayuda ndiponso anthu a mitundu ina okhulupilila amene Mulungu anawasankha kukhala mtundu wapadela ‘ kuti alengeze makhalidwe abwino kwambili ’ a amene anawaitana . Ndine wotsimikiza kuti Baibulo linandipulumutsa . 7 : 3 , 4 . 54 : 17 . Pamene tikambilana zina mwa zifukwazo , mungapeze mfundo zina za m’Baibo zimene nthawi zambili simuzigwilizanitsa na ciyembekezo canu cakuti okondedwa anu adzauka . 9 : 1 , 2 , 21 ; 10 : 20 - 24 ) Koma posapita nthawi , anayamba kucita zinthu modzitama . Tingathe kucita zimenezi kaya tili ndi zinthu zambili kapena zocepa . — 1 Mbiri 22 : 14 ; 29 : 3 - 5 ; Luka 21 : 1 - 4 . Ngati timatelo , ndiye kuti sicidzakhala covuta kugonjela m’dziko latsopano pamene Yehova azidzadziŵitsa mtundu wa anthu zimene amafuna . — Miy . Dziŵani zimene Nyimbo ya Solomo imatiphunzitsa ponena za cikondi ceniceni . Zimatenga nthawi kuphunzila bwinobwino cinenelo , koma muyenela kuwathandiza mwacikondi mmene angachulile bwinobwino mau . Atamasulidwa , Atate anayamba utumiki wa nthawi zonse monga kopotala ( mpainiya ) . 29 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi Nanga zimenezi zatithandiza bwanji pa nchito yathu yolalikila ? Tsopano , sindilekelela mkazi wanga kugwila nchito yekhayekha kukhichini . Timalambila Yehova . Kodi mungakonde kuphunzila Baibulo kwaulele ? Ndiyeno , m’caka ca 36 . Aliyense wa ife afunika kudzifunsa kuti , ‘ Kodi nimamvela malangizo a kapolo wamene Yesu akum’gwilitsila nchito ? Komabe , mwamuna amene wavulaza mai wongobeleka kumeneyo anali ‘ kumulipilitsa malinga ndi zimene mwiniwake wa mkaziyo angagamule . Mwacionekele , zocitika zina zidzayamba pamene zina zikali kucitika . Ngakhale m’magawo amene amalalikidwa kwambili timapezabe anthu amene amafuna kumvetsela uthenga wokondweletsa wa cipulumutso . Baibulo limati : ‘ Dziŵani bwino maonekedwe a ziŵeto zanu . ’ Iwo anadziŵa kuti Yesu anali kupemphabe Atate wake kuti amuthandize ngakhale kuti anali wangwilo . Baibulo limati : ‘ Mngelo wa Yehova anamupeza . ’ Tinazindikila kuti apolisi anali kufufuza m’nyumba za abale tsiku na tsiku . Conco , akuluwo analangiza Paulo kupita ku kacisi ndi kucita zinthu zimene zikanathetsa mabodzawo . Kumeneko anali kukhala m’matenti , anapilila ndi njala , ndipo anakumana ndi acifwamba . Mu August 2002 , ine ndi Susan anatiitana kuti tikatumikile ku Beteli ku Patterson , m’dziko la United States . ( b ) Ndani amene ayenela kugwilitsila nchito uphungu wakuti : “ Kumbukila Mlengi wako Wamkulu ” ? N’ciani cina cimene tifunika kucita kuti tione Mulungu ? ( Mat . 25 : 15 ) Ngakhale kuti mbuye anapatsa akapolo ciŵelengelo ca matalente cosiyana , iye anali kufuna kuti akapolo onse acite khama pogwilitsila nchito matalentewo . Mfumu Yesu Kristu ndi amene wakwela pahachi cifukwa ca cilungamo . 2 : 8 ) Nayenso Paulo anati : “ Cilamulo cimakwanilitsidwa m’cikondi . ” ( a ) Tingacite bwanji zinthu mogwilizana ndi pempho lathu lakuti Yehova atilanditse kwa woipayo ? Kwa George ndi Adria , kutumikila ku malo osoŵa kunawathandiza kudziŵa mmene kukhala amishonale kumamvekela . Conco , Luka akuonetsa mzele wobadwila wa Yesu “ monga munthu ” kupitila mwa Mariya , amai ake omubeleka . Akulu - akulu a asilikali ananena kuti adzapambana nkhondo mwamsanga ndi mosavuta , koma si mmene zinthu zinayendela . Ulosi umenewu unakwanilitsidwa pamene Mulungu anacotsa tembelelo pa nthaka . Koma zocitika za m’nkhani imeneyi zimatiphuzitsanso zinthu zina . 4 : 22 - 26 ) Mofananamo , cihema , kacisi , Tsiku la Mwambo Wophimba Macimo , mkulu wansembe , komanso mbali zina za Cilamulo ca Mose , zinali ‘ mthunzi cabe wa zinthu zabwino zimene zinali kubwela . ’ ( Aheb . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana zinthu zina zimene zatithandiza kulalikila uthenga wabwino padziko lonse masiku ano . Kukamba zoona , zidzakhala zosangalatsa kuona mmene Yehova adzaukitsila akufa . Zinaoneka kuti Aroni anasocetseledwa ndi anthu oipa . Komabe , pali zofalitsa zina zimene amalembela anthu monga acinyamata kapena makolo . Tikufunitsitsa kudziŵa mayankho a mafunso amenewa . Conco , tiyeni tipitilize kupenda lemba la Salimo 45 . Malinga ndi kafuku - fuku wina , kupatsa “ kumacititsa kuti munthu azikhala wacimwemwe , azigwilizana ndi ena , ndi kuwakhulupilila . ” Uŵaphunzitse ana . ” Mmodzi wa iwo ni Yosefe , mwana wa Yakobo . Pamene Timoteyo anali na zaka pafupi - fupi 20 kapena kupitililako pang’ono , analolela kudulidwa pofuna kuti asakakhumudwitse Ayuda amene anali kukawalalikila . Ngakhale kuti amayesetsa kuwayankha momveka bwino ndi mosamala , ena mwa anthuwo amawauza kuti , “ Pepani , koma nidziŵako munthu wina amene angakufunileni mankhwala . ” 32 : 17 - 20 , 26 . Tisaiŵale kuti pamene tithandiza abale athu , timakhalanso ndi cimwemwe cimene cimabwela cifukwa copatsa ena zinthu . Mwacitsanzo , banja lina linafikila mmishonale amene anali kuwaphunzitsa Baibulo ndi kumuuza kuti akufuna kukhala ofalitsa osabatizidwa . Iye sanaŵasungile cakukhosi . Patapita nthawi , Yosefe anapatsidwa mlandu wabodza ndi kuikiwa m’ndende . Mwacitsanzo , kodi munadzifunsapo kuti , ‘ N’cifukwa ciani tili ndi moyo ? ’ M’nthawi ya atumwi , bungwe lolamulila linatumiza kalata kwa abale m’mipingo yowadziŵitsa zinthu zina zimene anafunika kupewa . Palibe aliyense amene anali kuseŵenzetsa Baibulo , ngakhale kukambako za Mulungu kapena za Yesu . Ine ndi mkazi wanga , Merete , tinapitiliza kutumikila m’dela ndi m’cigawo mpaka mu 1976 . Komanso si bwino kupita pa Mawebusaiti kapena pa malo ocezela pa Intaneti osadziŵika bwino amene angationetse zinthu zaciwelewele ndi zamalisece . Ayuda atalimbikitsidwa na Mulungu , mosazengeleza anayambanso kugwila nchito yomanga ngakhale kuti inali ikali yoletsedwa . Kukhululuka kumatanthauza kuiŵalako zimene wina watilakwila na kusasunga cakukhosi . Kwa zaka zambili , Yehova wathandiza “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” kukhala wanzelu kwambili , kapena kukhala maso . Koma Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse itatha , padziko lapansi panalibe mtendele weniweni . Patapita cabe miyezi 6 kucokela pamene anapezeka pa msonkhano wa cigawo , iye anakamba nkhani yake yoyamba yoŵelenga Baibo ku Nyumba ya Ufumu . Baibo imaonetsa kuti panthawi ina , angelo anathandizapo alambili oona pofuna kukwanilitsa cifunilo ca Mulungu . N’cifukwa cake Yesu anawacha mabwenzi . Baibulo ndi buku lakale kwambili . 1 : 19 - 25 ) Mateyu analembanso zimene mngelo analamula Yosefe kupitila m’maloto zakuti athaŵile ku Iguputo , ndi mmene iye anathaŵila pamodzi na banja lake . Cinanso , analemba kuti kupitila m’maloto , mngelo anamuuza kuti abwelele ku dziko la Isiraeli . Analembanso za kubwelela kwake , na zimene anasankha zakuti akakhale ku Nazareti na banja lake . ( Mat . Kodi Mau a Mulungu amatithandiza bwanji kukulitsa cikondi cathu pa iye ? 4 : 9 ) Inde , cikondi n’cimene cinasonkhezela Mulungu kucita zimenezi . Mu 1992 , n’naikidwa kuti nizitumikila monga mkulu , ndipo n’nali m’bale woyamba wacikigizi kukhala mkulu mu Kyrgyzstan . Zina mwa zocitika zimene zili ka bokosi zinacitikapo ndipo zikucitikanso . Ganizilani za kusadalilika kwake . M’mau ena tingakambe kuti , tikadziikila colinga ca kuuzimu , tiyenela kukondwela ndi zimene ticita kuti tikwanilitse colinga cathu . Gulaye cinali cida cokhala na kathumba kakang’ono pakati pa nthambo ziŵili za cikumba , ndipo cinali cida cothandiza kwambili kwa m’busa . Iye anauza Abulahamu kuti nthawi zonse akamapeleka ciweluzo , amafufuza anthu abwino ndi kuwapulumutsa . — Genesis 18 : 22 - 33 . Colinga cake cacikulu cimeneci cimaonetsa cikondi ca Mulungu pa anthu , ndipo sicidzalephela olo pang’ono . MALINGA n’zimene tinakambilana m’nkhani yapita , Mdyelekezi amakamba kuti Yehova si wolamulila wabwino . Amakambanso kuti anthu angakhale na umoyo wabwino ngati adzilamulila okha . 4 : 8 ) Sitingathe kulemba mndandanda wa zifukwa zonse zimene timakondela Mulungu . Kodi simungandiuze cabe zimene limakamba ? ’ Kodi munakhalapo na mwayi woitanidwa ku nyumba kwa munthu wina kuti mukaceze ? Nanga tiphunzilapo ciani pa nsembe zimene Aisiraeli anali kupeleka ? Ndipo tingawakumbukile bwanji “ amene akutsogolela ” pakati pathu , makamaka amene amapanga “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu ” ? — Aheb . Mulungu anamulonjeza tsogolo labwino . Ndipo mwa thandizo la Yehova , takhala tikupambana . Patsogolo pake panalinso zolefula zambili , komanso kugonjetsedwa pankhondo . Timakumana pamodzi kuti tilambile Mulungu : Timakonda Yehova ndiponso timafuna kumumvela . Conco timafuna kumutamanda pamodzi ndi abale athu . Nthawi zina , tingacite bwino kukambilana mapemphelo amenewa pa nthawi ya kulambila kwa pabanja . Mkhristu aliyense analawako ubwino wa Yehova . Motani ? M’madela ambili anthu amakhalako ndi moyo wautali masiku ano kuposa zaka 100 zapitazo . 27 : 55 ; Luka 8 : 3 . Tili na zitsanzo zambili zoonetsa mmene Mau a Mulungu , mzimu woyela , ndi mabuku athu zathandizila Akhiristu kugonjetsa zilakolako zoipa . Yesu anali kukonda kwambili ophunzila ake cakuti pa ulaliki wake wa pa phili anacita kuwacenjeza ka 4 za kuopsa kodela nkhawa zinthu zosafunika . — Mat . Zioneka kuti akazi amenewa anali kugwilitsila nchito ndalama komanso katundu wao kuthandiza Yesu ndi ophunzila ake . Mwacitsanzo , ngakhale kuti Anna anali kutumikila mokhulupilika pa kacisi , mwina iye sanadziŵe kuti citsanzo cake cidzalimbikitsa ena mtsogolo . Amadziŵa kuti anthu amene amadalila Mulungu mwa kutsatila mfundo za m’Baibo ndiwo amapeza citetezo ceni - ceni ndi cokhalitsa . — Sal . Asayansi atafufuza , anapeza mapulaneti ena ambili . Ndi nchito iti imene a “ nkhosa zina ” amathandiza Isiraeli wa kuuzimu ? M’baleyo atamupempha kuti amuonetse mmene timaphunzilila Baibulo , iye anavomela . Ngati sitiloŵelela m’ndale , timaonetsa bwanji kuti tili ku mbali ya ulamulilo wa Yehova ? Koma tikamvela Yehova timaonetsa kuti tikufuna kuti iye azitilamulila . Mmodzi mwa abale amene anali kubwela kaŵili - kaŵili ndi mng’ono wanga Grigory , amene anatumikila monga woyang’anila woyendela kuyambila mu 1970 mpaka 1995 . Nanga bwanji za inu ? — Akolose 2 : 6 , 7 . Kodi mwatsimikiza mtima kucita ciani ? Iye anacita kumanga maguwa ansembewo pa phili loyang’anana ndi mzinda wa Yerusalemu , kumene anamangako kacisi wa Yehova . Ndiye cifukwa cake iye anapitiliza kunena kuti : “ Ambuye adzandipulumutsa ku coipa ciliconse . ” 25 : 4 . 5 : 17 , 18 ) Mukatelo mudzapeza mapindu ambili . mu Galamukani ! ya March 2012 , ikupezekanso pa webusaiti yathu ya www.jw.org . Mtumwi Paulo ananena kuti anali “ aulemelelo . ” 4 : 29 . Zimene okhulupilila zakuthambo amalosela masiku ano , zimazikidwa pa cikhulupililo cakale cakuti mapulaneti amazungulila dziko . Mfumu Davide , anakumana na mavuto ambili , koma Mulungu anam’pulumutsa . N’cifukwa cake iye anakamba kuti : “ Talaŵani ndipo muone kuti Yehova ndi wabwino . Wodala ndi munthu wamphamvu amene amathawila kwa iye . ” ( Sal . Masukulu amenewa aphunzitsa abale ndi alongo ndi kulimbitsa cikhulupililo cao . Komabe , anthu amene anafa ndi kupita ku “ kudziko la mdani ” wathu imfa adzamasuka ku ukapolo wa mdani ameneyu pamene akufa adzaukitsidwa . — Yer . Kulembedwa dzina ‘ m’buku la cikumbutso ’ la Yehova monga anthu ake kumabwela na udindo wake . Ndingasinthe ciani kuti ndikhale ndi tsogolo labwino ? ’ Mwacitsanzo , anandithandiza kuti ndisamacite mantha polalikila kunyumba ndi nyumba . ( Mac . Ndi cozizwitsa citi cimene mufuna kudzaona Yesu akucita mtsogolo ? Ndiye cifukwa cake Yehova wapatsa akulu udindo wophunzitsa ena mumpingo . ( 2 Tim . Mwacitsanzo , pa Sondo pa Nisani 9 , Yesu analoŵa mu Yerusalemu atakwela pa bulu . Yehova ndiye analamula . ( Mat . 13 : 18 , 19 , 22 ) Anthu ena amakhala ndi nkhawa nthawi zonse cifukwa cofunafuna ndalama kapena zinthu zina . Zinthu zonse za pa webusaiti yathu n’zotetezedwa mwalamulo . 11 : 5 ) Kodi zimenezi zinacitika bwanji ? NYIMBO : 121 , 45 5 : 3 ) N’zoona kuti nthawi zina , cingativute kucita phunzilo la umwini lopindulitsa cifukwa cotangwanika na zinthu zina . Panthawiyo , m’nyuzipepa ina analemba kuti a Mboni amakamba kuti afuna ng’ombe zogula , koma m’ceni - ceni amafuna nkhosa . 2 : 20 ) Komabe , zimene Yesu anacita pambuyo pa imfa ndi kuukitsidwa kwake , n’zimene zinacititsa kuti kukhale kotheka kuti macimo athu akhululukidwe . Mukacita conco , ‘ simudzakhala na mlandu wa magazi . ’ Ndiyeno Davide afunsa kuti : “ Ndani lelo ali wokonzeka kupeleka mphatso kwa Yehova ? ” Munthu aliyense amalakalaka kukhala ndi moyo wosatha . Timatha kugwila nchito yolalikila padziko lonse cifukwa cakuti ndife ogwilizana 8 Kodi Mumathaŵila kwa Yehova ? Mau Aciheberi ndi Acigiriki amene anamasulidwa kuti “ soul ” m’Cingelezi analinso ovuta kuwamasulila m’zinenelo zina . M’dzikolo munali msokonezo cifukwa anthu anali kumenyana , kuba , kugona anthu mwacikakamizo , ndiponso kuphana . Yosefe anafotokozanso kuti sanalakwe ciliconse ngakhale kuti anali m’ndende . Baibulo lili ndi mphamvu za Mulungu zogwetsa nazo “ zinthu zozikika molimba , ” kuphatikizapo mabodza ndi maganizo olakwika . ( 2 Akor . Tidzaonanso mmene kukhululukila ena akatilakwila mumpingo , kumaonetsela kuti timagwilizana ndi cilungamo ca Yehova . Mulungu kudzela mwa womulankhulila , analosela za kuonongedwa kwa mzinda wa Nineve . Kuwonjezela pa zimene Vicent anakamba zokhudza banja lawo , iye anakambanso kuti : “ Cifukwa ca kuŵelenga Baibo , manje nimaona kuti nili pafupi maningi na Yehova kuposa kale . ” 15 N’cifukwa Ciani Tiyenela Kusonkhana ? Msonkhano wacigawo mu 1941 , ku Mexico City Kumpoto kwa kacisi wa ku Yerusalemu kunali dziwe lochedwa Betesida . Iwo anacita zonse zotheka kuti akwanilitse zolinga zawo . Anthu amaseŵenzetsa mauthenga osoceletsa pofuna kupusitsa anzawo kapena kulamulila maganizo awo ndi zocita zawo . M’nkhani ino , tikambilana mau olimbikitsa a Yesu amene anakamba pa Ulaliki wake wa pa Phili wolembedwa pa Mateyu 6 : 25 - 34 . ( Salimo 40 : 5 ; 92 : 5 ; 139 : 17 ) Kuona zinthu mmene Yehova amaonela kumaticititsa kukhala anzelu , ndipo kudzatitsogolela ku moyo wosatha . — Ŵelengani 2 Timoteyo 3 : 14 - 17 . M’Paradaiso ameneyu timakhala otetezeka ngakhale kuti tili m’dziko loipa . Malinga ndi mau a lemba limene tagwila mau kumayambililo a nkhani ino , Yehova amakokela anthu kwa iye . 2 : 5 - 8 ) Kodi si zolimbikitsa kudziŵa kuti abale na alongo athu akwanitsa kupilila mavuto osiyana - siyana mu umoyo wawo mothandizidwa na Mau a Mulungu ? Baibulo limati : “ Ndiyeno Farao anauza Yosefe kuti : ‘ Ine ndalota maloto , ndipo palibe munthu amene wakwanitsa kuwamasulila . Mulungu akaloŵelelapo pa zocitika zimenezi , zingatanthauze kuti amadziŵilatu zinthu zoipa zisanacitike . Kodi uthengawu ukukhudza odzozedwa okha ? 4 : 8 , 9 ) Koma kumbukilani kuti Yehosafati anavomeleza pa gulu la Aisiraeli kuti iye ndi anthu ake analibe mphamvu . Kodi anthu ambili opita kukagwila nchito ku maiko ena amakumana ndi mavuto ati akabwelako ? Henry , amene watumikila monga woyang’anila kwa zaka zambili anati : “ Ngati mukukalamila , yesetsani kugwila nchito mwakhama kuti muonetse kuti mukuyenelela . ” 8 KUTI MUNTHU AKHALE MTUMIKI WACIKHRISTU , KODI AFUNIKA KUKHALA WOSAKWATILA ? Tikamapilila mavuto amene tikumana nao m’dziko lino , timaonetsanso kuti tili ndi cikhulupililo mwa Yehova . “ Ndinali kufunitsitsa kudziŵa mmene akufa alili . 24 : 29 - 31 ) ‘ Kusonkhanitsa osankhidwa ’ kochulidwa pa lembali , kudzacitika pa nthawi imene Akhristu odzozedwa onse amene adzakhala akali pa dziko lapansi adzalandila mphoto yawo ya kumwamba . Yehova anali atauza mwamuna wake kuti : “ Ndidzamudalitsa ndipo iwe ndidzakupatsa mwana wamwamuna wocokela mwa iye . Ndipo monga mmene taonela , zipatso zimene mmela wa tiligu umabala si tummela twatsopano tung’ono - tung’ono . Koma umabala mbewu . Tingakambe mosaganiza bwino kapena kucita zinthu panthawi yolakwika . Mwina tinganyalanyaze zinazake kapena kuiŵala . Koma kumbali ina , Davide anadziŵa kuti Yehova adzam’konzekeletsa Solomo kuti ayendetse bwino nchitoyo . Baibulo limalimbikitsa Akristu oona kusapeputsa mphamvu ya pemphelo . Timalimbikitsidwa . 11 : 7 . Acinyamata ambili ali ndi maudindo ocepa m’banja , ndipo ali ndi thanzi ndi mphamvu cakuti angakwanitse kugwila nchito zovuta . Yehova anatumanso mngelo kukalimbikitsa Yesu atavutika maganizo usiku wakuti mawa aphedwa . Pamene muwonjezela luso ndi kukhala na cidalilo polalikila , kupita kwanu patsogolo kudzaonekela . ( Aroma 1 : 14 , 15 ) Kukumbukila mfundo imeneyi kuyenela kutilimbikitsa kuuzako ena uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu . — Sal . Muyenelanso kuphunzila nkhani imeneyi ndi zina zokhudzana ndi imeneyi pa phunzilo lanu laumwini kapena pa kulambila kwa pabanja . Ndipo makope oyambilila okwana 1,200 amene anapulintiwa , anasila pambuyo pa miyezi yocepa cabe . Ndinadabwa kwambili pamene io anandionetsa dzina la Mulungu lakuti Yehova m’Baibulo langa la Cihangare . Tikamacita zimenezi , nyumba zathu ndi Nyumba za Ufumu zidzakhala malo acimwemwe na citetezo . Cimadalila mpweya wotentha , umene umacithandiza kuulukila m’mwamba popanda kuwononga mphamvu zambili . Yehova anaonetsa kuti ni wapamwamba kwambili kuposa milungu yonama imeneyo pamene anabweletsa Milili 10 . Poyamba , liu lakuti “ tuakacisi ” linali kuimila malo amene anali kuikapo zinthu zopatulika zacipembedzo . M’modzi wa iwo anali Eunice Colin , amene n’nakumana naye koyamba pa sukuluyo pamene n’nali kutsiliza maphunzilo anga . Ndipo anali kugwilitsila nchito ufa wosalala wa ku dela kumene anali kukhala panthawiyo . Pamene Paulo anakamba mau amenewa , anaonetsa kuti kupita patsogolo kuuzimu kumafuna khama . Pamene Yesu anamulola kupita kwa iye , Petulo anatuluka m’bwato ndi kuyamba kuyenda pamadzi . Kaya ndife abale kapena alongo , tonse tiyenela kucita zimene tingakwanitse kuti tizigwila nchito iliyonse imene tapatsidwa . Yesu anaonetsa mtumwi Yohane masomphenya a “ mkwatibwi , ” amene ndi odzozedwa okwana 144,000 omwe adzalamulila ndi Kristu kumwamba . Iwo anali kuitana anthu kuti “ amwe madzi a moyo kwaulele . ” ( Chiv . 4 : 23 , 24 ) Mwacionekele , inunso mungavomeleze kuti panthawi ya mavuto , kukhala ogwilizana n’kofunika kwambili . Amy , wa ku United States , amene lomba ali ndi zaka za m’ma 30 , anayankha kuti : “ Kwa zaka zambili , n’nali kufuna kukatumikila ku dziko lina losoŵa , koma n’nali kuona monga siningakwanitse . ” M’pempheni kuti akuthandizeni kucita zinthu zoyenela pa zocitika zotelo . Koma tinadabwa kwambili titafika ku nyumba . N’ciani cimene muyenela kuphunzitsa ana anu ? Nanga mungacite bwanji zimenezo ? Akanani anali otsimikiza kuseselatu adani ao mosavuta ndi mofulumila kwambili cifukwa analibe mphamvu . — Oweruza 4 : 12 , 13 ; 5 : 19 . Yehova . Conco , anakonza ciwembu mwa ‘ kupangitsa malamulo ’ oyambitsa mavuto . Ndinali ndi mwai wapadela kutulutsa Baibulo la Dziko Latsopano Lomasulira Malemba Achigiriki Achikhristu m’Cituvalu . ( a ) Kodi Salimo 34 : 22 imaonetsa bwanji kuti atumiki a Mulungu safunika kumangodziimba mlandu ? ( Mac . 17 : 28 ) Yehova anatipatsa dziko lapansi lokongola kwambili monga malo athu okhala . ( Sal . 4 Mauwa ni olimbikitsanso kwa anthu a Mulungu masiku ano . Caciŵili , tiyenela kusamala kuti tisamangoyang’ana zimene timacita bwino pa umoyo ndi kunyalanyaza zimene timafunikila kukonza . Iye ndi wacilendo ndipo akukufunsani kuti adziŵe zakudya zimene mukonda . Mabaibulo amenewa analembedwa kale kwambili , zaka 200 Kristu asanabadwe , ndipo ena analembedwa zaka 100 Kristu atabadwa . Iwo anali osweka mtima , ndipo anafunika kutonthozedwa . Yehova anadalitsa Yefita ndi Aisiraeli cifukwa ca mmene Yefita anacitila zinthu . — Aheberi 11 : 32 , 33 . Pamene n’naponda pa mitengoyo , inagwela mkati , ndipo inenso n’nagwela momwemo . TSAMBA 21 • NYIMBO : 26 , 89 Koma anadziŵa kuti Kristu sanafele anthu angwilo , koma ocimwa monga iye . Ndinaona monga zonse zathela pamenepa , ndipo ndinali ndi mantha kwambili . ” Yesu anali kukhudzidwa kwambili ndi mavuto a ena . Iye anakamba kuti sakumbukila zonse zimene m’bale ndi mlongoyo ananena , koma anali kukumbukila kwambili kukoma mtima kumene io anaonetsa kwa iye . Ngati zinalidi conco , ndiye kuti iye anapatsidwa mwayi wokakhala na Yesu kumwamba kwamuyaya . Ndithudi ! Mofulumila anthu onse anayamba kuthaŵila ku mapili , uku akukuwa kuti “ Smong ! Iye anafunikila kuiŵala zolakwa zao ndi kulimbikitsa mgwilizano mumpingo . Posinkhasinkha coonadi ca mtengo wapatali cimeneco , munaphunzila mmene mungakhalile bwenzi la Yehova . ( b ) Nanga Abulahamu anaika maganizo ake pa ciani ? Iye adzayankha pemphelo lathu lopempha cikhulupililo coonjezeleka , cikhulupililo cathu cidzalimba kwambili , ndipo tidzakhala “ oyenelela Ufumu wa Mulungu . ” — 2 Atesalonika 1 : 3 , 5 . Conco , tingaone zimene tikuphunzilapo pa nkhani ndi zocitika zochulidwa m’Baibulo , m’malo mofotokoza zinthu zimene nkhanizo zimaimila . Olo kuti simungasinthe zinthu zimene zinacitika kale , pali zimene mungacite kuti imwe na okondedwa anu mukhale na tsogolo labwino . Kumeneko mabomba ndi maloketi anali kungokhalila kuphulika . Baibulo la Septuagint likali lofunika masiku ano cifukwa limathandiza akatswili kumvetsa mau ndi mavesi ovuta aciheberi . Izi zisanacitike , Petulo anali atakana Yesu katatu cifukwa ca mantha . ( b ) Kodi Yehova anapanga makonzedwe otani kuti ayeletse dziko lapansi ndi kuteteza anthu ? Yehova ndi Yesu saona kuti mtundu wina , dziko lina , kapena cinenelo cina ndi zapamwamba kuposa zina . ( Mac . 10 : 34 , 35 ; Chiv . Mu 1939 , nkhondo yaciŵili ya dziko lonse inayamba . Caka cotsatila , nchito ya Mboni za Yehova inaletsedwa m’dziko la Canada . ( 2 Petulo 3 : 9 ) Iye akupatsa anthu mwai wovomeleza Yesu kukhala Wolamulila wao . Ndinabatizidwila ku Queensland , ndinasangalala kucita upainiya ku Tasmania komanso umishonale ku Tuvalu , ku Western Samoa , ndi ku Fiji Abalewo atakhala okhaokha , m’bale amene anakhumudwa anayamba kudandaula za mlongoyo . Conco , pamene mukamba kuti “ pepani ” kwa mnzanu wa m’cikwati komanso kwa ana anu ngati mwalakwitsa , ndiye kuti mupeleka citsanzo cabwino cokhala oona mtima ndi odzicepetsa . Sitiyenelanso kucita nsanje olo kuti tinam’thandiza pa zimene anacitazo . 13 : 18 . Satana ananeneza Yobu , munthu wolungama uja , na kumubweletsela mavuto aakulu kuti amufooketse . Koma ciwembu cake cinalephela . Yosefe analila cifukwa ca zimenezi . 10 , 11 . ( a ) Tingatengele bwanji citsanzo ca atumiki a Yehova akale amene anali owoloŵa manja ? Akazi Acikristu ayenela kutsatila khalidwe lake labwino limeneli . Pamene masiku otsiliza anayamba mu 1914 , panali atumiki a Mulungu ocepa cabe . Mwa cilolezo ca Abulahamu ndi thandizo la Mulungu , Sara anadzudzula Hagara mwamseli . Inu mungadabwe kuti , ‘ Kodi padziko lapansi pakhalako mtendele woculuka bwanji ? ’ Nanga zocitika zimaonetsa ciani ? Nthawi zina anali kuponya manja ndi miyendo yake mwadzidzidzi cakuti anali kudzivulaza . Amaganiza kuti Mulungu anaseŵenzetsa cisanduliko kupanga zinthu zosiyana - siyana . 4 : 6 ; Luka 11 : 13 ) Nchito imeneyi yakhala ndi zotsatilapo zabwino monga mmene Buku Lapacaka la Mboni za Yehova limasonyezela . ( Yobu 14 : 15 ) Ganizilani cimwemwe cimene tidzakhala naco polandila anthu oukitsidwa padziko lapansi . imathandiza bwanji kuyeletsa dzina la Yehova ? Dzuŵa ndi imodzi mwa nyenyezi zimene zili mu mlalang’amba wathu wa Milky Way . 24 : 15 ) Ngati tasankha njila yabwino , tingayang’ane kwa Yehova kuti atsogolele mayendedwe athu . N’nali na mwayi wokumana ndi amishonale akale amene analoŵa makilasi oyambilila a Sukulu ya Giliyadi , ndipo anali kutumikilabe mokhulupilika m’maiko amene anatumizidwa . Mwacitsanzo , ca m’ma 100 C.E . , Akhiristu a mu mzinda wa Efeso anashoka mabuku awo onse a zamatsenga . 2 : 12 ) Ngati munthu ali na udindo waukulu , Yehova amayembekezelanso zambili kwa iye . ANTHU SADZAKOKANSO FODYA Baibulo linathandiza Olaf , Jayavanth , ndi Armen kuleka cizoloŵezi coipa cimene cinali kuwaononga ndi kuononga anthu ena . M’malo mwake , “ amapemphela kuti atonthozedwe basi . ” 2 : 2 ) Conco , tisaleke kucitila umboni . ( Mlaliki 9 : 11 ) Pamene zinthu zosayembekezeleka kapena ngozi zacitika , kaya wina wakhudzidwa ndi zocitikazo kapena iyai , zimadalila kwambili malo amene munthuyo anali pamene ngoziyo inali kucitika . Nkhani ya Yobu imapeleka umboni wakuti “ Yehova ndi wacikondi cacikulu ndi wacifundo . ” 18 “ Usacite Mantha . mwana woloŵelela ? M’malo mwake kuukila kwao kudzaimitsidwa kwakanthawi . ( Sal . 118 : 6 ) Ni mwayi wamtengo wapatali kwambili kukhala kumbali ya Mulungu , ndi kukhala naye pa ubwenzi wabwino . ( b ) Kodi Malemba amalangiza ana kucita ciani ? 14 Mzimu Umacitila Umboni Limodzi ndi Mzimu Wathu Kuphunzitsa ana kungakhale kovuta kwambili ngati mnzanu wa m’cikwati ni wosakhulupilila . Mukhozanso kukonza zoti mukadzamwalila , gulu la Mulungu lidzatenge zinthuzo . NYIMBO : 82 , 77 Ndi fanizo liti limene lionetsa kuti sikwanzelu kukhulupilila kuti Mulungu anaika Mdyelekezi kuti azizunza anthu m’moto wa helo ? Pa lemba la Aroma caputala 16 , Paulo anayamikila okhulupilila anzake oposa 20 cifukwa ca makhalidwe ao abwino . 3 : 24 ) Ndipo buku la Chivumbulutso 22 : 6 , limaonetsa kuti Yehova “ anatumiza mngelo wake kudzaonetsa akapolo ake zinthu zimene ziyenela kucitika posacedwa . ” Kodi n’ciani maka - maka cimene cimawakondweletsa ? Sikuti odzozedwa amenewa anangomasulidwa m’ndende cabe , koma amene anakhalabe okhulupilika analandila udindo wapadela wocokela kwa Mulungu kupyolela mwa Mbuye wao Yesu Kristu . Cinanso , kulemekeza ena moyenelela kumatithandiza kuti tiziyendela pamodzi ndi gulu la Yehova , limene limapewa kutamanda anthu mopambanitsa , kaya ni Mboni kapena ayi . Koma n’naphunzila m’Baibo kuti Mulungu amazonda anthu amene amalambila “ mulungu wa Mwayi , ” komanso anthu adyela . Kucita zimenezi kudzatithandiza kukonda kwambili coonadi ca m’Baibo . — Ŵelengani Salimo 1 : 2 . “ Mudzamva phokoso la nkhondo ndi mbili za nkhondo . Izitu zisadzakucititseni mantha . Munthu amene afuna kutumila ena nkhani angalephele kuona kaya nkhaniyo ndi yoona kapena ai , cifukwa kucita zimenezo kumafuna nthawi ndi khama . Khama lathu poteteza uthenga wabwino limacititsa kuti tipambane . N’cifukwa ciani tifunika ‘ kucita pangano ndi maso athu ’ ? Nanga tingacite bwanji zimenezi ? Ponena za nchito yomanganso kacisi , Yehova analonjeza kuti : “ Ici cidzacitika ngati mudzamvela mwacangu mau a Yehova [ Mulungu ] wanu . ” — Zek . M’malomwake , tifunika kuphunzila zimene Mulungu amafuna , ndi kusankha zocita mogwilizana ndi zimene taphunzilazo . Mafunde akuomba ngalawa mwamphamvu kwambili ndipo madzi ena akugwela m’ngalawayo pamodzi ndi vithovu . ( b ) N’cifukwa ciani ubatizo wacikhristu ni wofunika kwambili ? 2 : 3 , 4 ) Tikatelo , tidzathandiza anthu amene , monga Peter , ni osaoneka bwino m’maso mwa anthu , koma ali na mtima wabwino . ( Yoh . 8 : 48 ) Asamariya sanali a mtundu waciyuda , ndipo anali na cipembedzo cawo . Mulungu anaika mwamuna kukhala mutu wa mkazi wake . ( 1 Akor . ( 1 Mafumu 17 : 21 ) ( 4 ) Sanakaikilenso kuti Yehova adzanyeketsa nsembe imene iye anapeleka pa Phili la Karimeli . Mwacitsanzo , mumzinda wa Pietermaritzburg , ku South Africa , nyuzipepala ina imene imachedwa kuti The Witness yakhala ikufalitsidwa kwa zaka 160 tsopano . ( Afil . 2 : 3 ) Anatilenga na cikumbumtima , cimene ni luso lobadwa nalo , lotithandiza kudziŵa cabwino ndi coipa . Pofotokoza cizindikilo ca kukhalapo kwake , Yesu anakamba mafanizo aŵili amene tidzakambilana . Pa misonkhano , iye amayang’ana pa kompyuta moleza mtima kuti apeze kacizindikilo koyenelela , kenako mau ake ocokela m’kompyuta amamveka kwa onse . ( Dan . 10 : 8 , 11 , 18 , 19 ) Nanga imwe , simungalimbikitseko ofalitsa , apainiya , na okalamba mumpingo mwanu amene mphamvu zawo zikucepela - cepela ? ( Mac . 10 : 42 ) Timafunitsitsa kulengeza uthenga wabwino ndipo kucita zimenezi n’kofunika . 38 : 2 - 4 ) Panthawiyo , Gogi adzaukila “ anthu amene anasonkhanitsidwa pamodzi kucokela ku mitundu ina , ” amene ndi anthu a Yehova . ( Ezek . Tsiku lina , ali pabedi , ananipempha kuti nimuŵelengele zofalitsa zina zimene zinali kufunika kupulintiwa . Yaeli anam’funditsa bulangete ndipo atam’pempha madzi akumwa , anam’patsa mkaka . Anthu ambili amakhulupilila kuti angelo aliko , ndi kuti amawathandiza . Munthu wina akatilakwila , amakhala ndi ngongole kwa ife . NYIMBO : 117 , 114 Conco , sitiyenela kukhala na maganizo akuti munthu payekha angadziŵe zabwino na zoipa popanda kukhulupilila Mulungu na kutsatila mfundo zake . — Sal . Molimba mtima , Inoki analengeza uthenga wocenjeza umenewu wocokela kwa Mulungu ali yekha - yekha . Iwo adzaweluzidwa mogwilizana ndi mmene akukwanilitsila udindo wao umenewo . Tikacedwa kuthetsa nkhani , cimakhala covuta kwambili kukhazikitsa mtendele na m’bale wathu . A Zimba : Eya , ndinali kufuna kufunsa funso limeneli . Abale na alongo amene anacokela ku maiko ena anasangalala kwambili kugwila nawo nchito yolalikila imeneyi . Kumbukilani kuti kuonetsa cidwi kwa alendo n’kothandiza nthawi zonse . 6 : 8 ) Nthawi zonse , Yehova amadalitsa anthu amene amayamikila mwai wogwila nchito ndi iye , mosasamala kanthu kumene akutumikila . Yehova analoŵelelapo kuti ateteze mkazi wokondeka ameneyu , mwa kugwetsela Farao ndi banja lake milili . Nchito yolalikila imeneyi ikucitika padziko lonse lapansi mothandizidwa ndi angelo . — Chivumbulutso 14 : 6 . Iye anakamba kuti tsiku lina amayi akewo anadziwonongela . “ Lilani Ndi Anthu Amene Akulila ” , July Pamene anali kubatizika , zinali ngati kuti akuuza Yehova kuti : “ Ndimakondwela ndi kucita cifunilo canu , inu Mulungu wanga . ” ( Sal . M’malomwake , mipukutu imeneyi yathandiza kuti Mabaibulo a masiku ano akhale olondola kwambili . Pokamba za Malemba Acigiriki Acikhiristu , Sir Frederic Kenyon analemba kuti : “ Palibe buku lina lakale limene lili ndi umboni woculuka ndi wodalilika wotsimikizila kuti zolembedwa zake n’zolongosoka . THANDIZANI ENA KUKHALA MABWENZI A YEHOVA Ku polisi ya ku Lilongwe anandicitila zinthu mokoma mtima . Kodi panali kusiyana kotani pakati pa Aisiraeli ndi asilikali a Yabini ? Onse anangoziona ngati zoseketsa , maka - maka Margaret , ndipo onse anadya zakudyazo popanda makaloni . Anafunika kuthaŵila ku mzindawo mwamsanga na kukhala kumeneko kuti ateteze moyo wake . Maganizo oipa akazika midzu mumitima ya anthu aŵili amene akhala akukopana , io angayambe kukambilana nkhani zimene ayenela kukambilana ndi mwamuna kapena mkazi wao cabe . 11 : 23 - 25 . Ikakhala mbali ya citsanzo , tonse tinali kuyenda kupulatifomu popanda omvetsela . M’kupita kwa nthawi , mlongo wacikulile anayamba kupezekapo . 2 : 4 ) N’cifukwa cimodzi citi cimene ciyenela kuti cinacititsa zimenezi ? Kodi ndi dziko liti limene linaonongedwa ? N’ciani cimene muyenela kucita ngati mwaona nkhani inayake pa Intaneti imene ionetsa mabodza amkunkhuniza okhudza gulu la Yehova ? Cinsinsi Namba 8 Citsanzo ( Luka 22 : 18 , 28 - 30 ) Komabe , Mkwati ndi mkwatibwi si ndiwo okha amene adzasangalala cifukwa ca cikwati ca Mwanawankhosa . Mwasintha n’kukhala wankhanza kwa ine . Ndi mphamvu yonse ya dzanja lanu , mwandisungila cidani . ” — Yobu 30 : 20 , 21 . Kodi angakhale na umoyo wabwino popanda ulamulilo wa Mulungu ? Timapindulanso kwambili na malangizo auzimu amene timalandila . Konzekelani Kudzakhala m’Dziko Latsopano Iwo anamwetulila na kunifunsa kuti “ Mudzabweladi ? ” Iwo sanabwelelenso kunyumba yao ku New York . Ndikanalekelela khalidwe loipa la mwana wanga , iye sakanabwelelanso . ” Ca kumapeto kwa ma 1800 , n’ciani cimene odzozedwa anacita kuti amvetse Mau a Mulungu molongosoka ? Kodi Isaki amene anali kudzakhala mwamuna wake anali munthu wotani , popeza anali asanaonanepo ? Zimene ndinaphunzila zinandithandiza kukhala munthu wabwino . ( Aef . 1 : 20 - 22 ) Monga Mfumu , Yesu amagwilitsila nchito mphamvu zake kuti ateteze ndi kutsogolela ophunzila ake ndi colinga cakuti cifunilo ca Atate wake cicitike . Kodi kukwanilitsika kwa ulosi wa Ezekieli kumaonekela bwanji pa Cikumbutso caka ciliconse ? Iye anati , “ Wamng’ono adzasanduka anthu 1,000 , ndipo wocepa adzasanduka mtundu wamphamvu . Kukamba zoona , Ophunzila Baibo amene analiko panthawi ya nkhondo yoyamba ya dziko Lonse ( 1914 - 1918 ) anacitila umboni motamandika . Anatinso : “ N’nali kudelanso nkhawa kusiya amayi amene anali kusamalila atate anga odwala . N’ciani cinathandiza Rhonda kupilila ? Iyai . Iye alibe makhalidwe abwino . Kafukufuku aonetsa kuti anthu amene sakhululuka . . . Ali nu ! kupitana - pitana ndi kukambitsana ndi anzawo . Timathandizidwa kupewa mayeselo “ Pemphelani kosalekeza , kuti musaloŵe m’mayeselo . ” — Luka 22 : 40 . Motelo , nthawi zina ena mumpingo angakambe kapena kucita zinthu zimene zingatikhumudwitse . Ndithudi , akufa adzakhalanso na moyo . 6 : 12 . Mfundo za m’Baibulo n’zimene ziyenela kutithandiza kusankha bwino mavalidwe . M’nthawi ya Yesu , cipembedzo nthawi zambili cinali kutenga mbali m’zandale . Ngati mwaona kuti n’zovuta kuuza munthu mau om’tonthoza pamaso - m’pamaso , mungam’patse khadi ya uthenga wacitonthozo , kumulembela meseji pafoni kapena pa kompyuta , kapena kumulembela kalata . Koma cifukwa cokonda kuthandiza ena , ndinali kutsogoza maphunzilo , kulimbikitsa abale pa Nyumba ya Ufumu , ndi kulalikila nao . ( Luka 6 : 38 ) Mukakhala opatsa , anthu adzayamikila kwambili khalidwe lanu limeneli , ndipo mudzawathandiza kuti naonso akhale opatsa . Abale ena aciheberi anacitila akazi amasiye acigiriki zinthu zopanda cilungamo . Nthawi zina , Paulo anali kulalikila anthu okhala na zikhulupililo zabodza zozika mizu kwambili . Kodi m’nkhani ino tidzakambilana ciani ? Tikayamba kufotokozelana zinthu zabwino zimene zinaticitikila , timalimbikitsidwa kwambili . ” 6 : 16 , 17 ) Kodi Malemba amaonetsa bwanji kuti kupanga malonjezo kwa Mulungu ni nkhani yaikulu ? Mau athu . Tiyenela kuyamikila Mulungu ndi kum’tamanda cifukwa ca cifundo cake . Nayenso Loti anapita nawo pomvela Yehova , ndipo iwo “ anasamuka m’dziko la Akasidi . ” — Machitidwe 7 : 4 . Tsikulo lidzakhala loyamikiladi Yehova . — Chiv . Coyamba , akuluwo anafunika kumvetsetsa zimene zinacitikazo . Nayenso woyang’anila dela ali ndi udindo waukulu wopenda mosamalitsa ndiponso mwapemphelo ziyamikilo zocokela kwa akulu , ndi kuika pa udindo abale amene akwanilitsa ziyeneletso . Kodi Cikomyunizimu cinangotiphimba pamaso ? Koma zimenezi n’zogwilizana ndi mau amene Yehova anakamba ponena za Gogi . Iye anati : “ Udzabwela kucokela kumalo ako , kumadela akutali a kumpoto . Udzabwela ndi mitundu yambili ya anthu . Anthuwo adzakhala khamu lalikulu , adzakhala cigulu cacikulu cankhondo . Onsewo adzabwela atakwela pamahachi . ” — Ezek . Tidzakambilana mbali zinayi zikulu - zikulu izi : anthu oipa , mabungwe acinyengo , makhalidwe oipa , ndi mavuto . 4 : 12 . Masiku ano , Yehova watiphunzitsa zinthu zambili zokhudza iye , colinga cake , cilengedwe cake , komanso Mau ake . Pamene maganizo anga anatsimikizila za mfundoyo , ndinatsimikiza za kumamatila ku gulu lokhulupilika . Mungacite ciani kuti mucepetseko nkhawa ? Anandiphunzitsa zambili ponena za Atate Woyela woona wakumwamba , Yehova Mulungu . ( Yoh . Kodi mmene munaleledwela kapena malo amene mumakhala zinali kukucititsani kukonda kwambili dela kapena dziko lanu ? “ Mulungu woona sangacite zoipa m’pang’ono pomwe , ndipo Wamphamvuyonse sangacite zinthu zopanda cilungamo ngakhale pang’ono . ” Iyai . Anayembekezela kuti mzimu wa Yehova umuthandize kudziŵa nthawi imene angayambe kusamalila udindo waukulu . Nikapita kukaona anthu kunyumba , ine na Arthur tinali kutsukila pamodzi mbale tikatsiliza kudya . Limbitsani cikhulupililo canu cakuti mapeto ali pafupi mwa kuŵelenga maulosi a m’Baibulo amene akuonetsa kuti tili m’masiku otsiliza . Monga mmene Baibo inakambila , anthu ambili masiku otsiliza ano ‘ safuna kugwilizana ndi anzawo . ’ Komabe , tonse timalakwa kaŵili - kaŵili . Mlongo ameneyu pamodzi ndi mwamuna wake Martinus , athandiza anthu ambili , kuphatikizapo ana ao atatu , kuyamba kulambila Yehova . Pamapeto pake , mukuthawa pakati pamseupo mwamsanga . Asilikali a zipembedzo zosiyana - siyana zacikristu analimbikitsidwa kupha anzao m’dzina la Mpulumutsi wao . ” — A History of Christianity . Pa Pentekosite , Petulo anauza Ayuda molimba mtima kuti afunika kukhulupilila Yesu , munthu amene io ‘ anamukhomelela pamtengo , ’ popeza “ Mulungu anamuika kukhala Ambuye ndi Kristu . ” Zoonadi , anthu ambili anaona kuti nchito yapadela inali kucitika . Kwa Ayuda okhulupilika , umoyo unali wovuta kwambili ku Babulo . Musaganize kuti Mulungu wakusiyani . Kodi kuganizila zoipa kungativulaze bwanji ? Anacepetsa nthawi yoseŵenza n’kuyamba kucita upainiya . Cinanso , anaganizila za cimwemwe cimene iye na mkazi wake angapeze ngati apita kukatumikila kumene kuli olengeza Ufumu ocepa . Nanga anakwanitsa bwanji kuphunzila Cimalagase ? Nanga bwanji ngati mwamuna kapena mkazi wanu wosakhulupilila akukuikilani malile pa kulambila kwanu ? Mafunso amenewa ndi ena adzayankhidwa m’nkhani ino . ( Salimo 34 : 14 ) Ngati tiyesetsa kukhala mwamtendele ndi ena , tidzakhala paubwenzi wabwino ndi abale ndi alongo athu , ndipo tidzakhalabe ogwilizana . Lefèvre sanalole olo pang’ono kuti anthu otsutsa am’lepheletse kumasulila Baibo . * Kumeneko , Aisiraeli anayambanso kudandaula cifukwa cosoŵa madzi . ( Num . Seŵenzetsani mpata ulionse . N’cifukwa ciani nthawi zina sitingaone dzanja la Yehova pa umoyo wathu ? 6 : 33 ) Pokhala alengezi a Ufumu ‘ tapatsidwa nchito yolalikila uthenga wabwino ’ ndipo Yehova amationa kuti “ ndife anchito anzake . ” ( 1 Ates . 2 : 4 ; 1 Akor . 3 : 9 . ) Kodi nkhani ino yakuthandizani bwanji ? Yelekezelani kuti mukuona mmene zinthu zinalili panthawiyo : Kristu watopa pambuyo polalikila kwa nthawi yaitali . Ndithudi , usiku impso zanga zandiwongolela . ” Sitidzacitila nsanje abale athu kapena kukhala aumbombo . Conco , dziŵani zimene mwana wanu wacinyamata amakonda , monga nyimbo , mafilimu , ndi maseŵela . Gwilitsilani Nchito Mau a Mulungu — Ndi Amoyo , 8 / 15 Iye sayenela kukalipila mlongoyo cifukwa covala mosayenela , koma angamulimbikitse kuganizila mmene kavalidwe kake kangakhudzile anthu ena . ( 1 Tim . Wapolisiyo anakalipa , amvekele : “ Kukhala wa Mboni ni mlandu waukulu kwambili kuposa wina uliwonse . ” Ni pa zocitika zina ziti pamene makolo acikhristu amafunika kukhala olimba mtima ? Cimodzi cimene tifunika kucita ni kuseŵenzetsa kwambili Baibo polalikila ndi pophunzitsa . Abuda ndiponso anthu amene amakamba kuti ndi Akristu , kuphatikizapo ena , amaona kuti palibe colakwika kucitako miyambo ya Cishinto m’kacisi ameneyu . “ Yehova , Yehova , Mulungu wacifundo ndi wacisomo . ” — EKS . Pa Sondo , anthu a ku Poland amene anali kugwila nchito kumigodi anali kuvala zovala zabwino popita ku chalichi monga mmene anali kucitila kwao . Cifukwa ca ici anthu ena a ku France anali kuwasuliza . Izi zingaphatikizepo kukhala chelu akaona zizindikilo zakuti wacicepele akupita patsogolo mwauzimu . Ukamatelo , ena nawonso azikumvetsela mwaulemu . ( Ŵelengani Aheberi 6 : 10 ; 11 : 6 . ) Iye amayamikila zimene mtumiki wake aliyense amacita , ndipo amaona kuti kunyalanyaza atumiki ake okhulupilika kungakhale kupanda cilungamo . Ndiponso padziko lapansi sipadzapezeka munthu wosauka , cifukwa ndico colinga ca Mulungu . — Yesaya 45 : 18 . Kulambila Kwa Pabanja , 3 / 1 Kulandila “ Cakudya pa Nthawi Yoyenela ” 8 / 15 Ngati zili conco , ndiye kuti zimene Malemba amakamba ponena za Timoteyo zimakhudzanso inu . M’bale Knorr anamwalila mu 1977 , koma onse amene anali kumudziŵa ndi kum’konda anatonthozedwa podziŵa kuti anatsiliza moyo wake wa padziko lapansi ali wokhulupilika . ( Chiv . Kodi anakhumudwa ? Iye adzapitiliza kuyenda nanu . Tingacite ciani kuti tikhalebe na “ mtendele wa Mulungu ” pamene takumana ndi mavuto ? Nanga kumasiyana bwanji ndi kunyadila ? “ Yehova Ndiye Mwini Nkhondo ” 9 Wofalitsa wina wosabatizika dzina lake Haykanush , amene amakhala ku Armenia anatola kacikwama ka ndalama pafupi ndi nyumba yake . Kodi si zoona kuti tonsefe timaona kuti zinthu zimenezi n’zofunika ? Matanthwe a ku Meriba woyamba ni a nsangalabwi ( kapena kuti olimba kwambili ) . Cifukwa ca macimo athu kwa Mulungu sitinali oyenela kukhala ndi moyo . . . . Zimenezi zinacititsa kuti Natanayeli asinthe mmene anali kuonela anthuwo . Kuonjezela apo , imodzi mwa njila zimene mungalimbitsile ubwenzi na munthu ni mwa kucitila naye zinthu pamodzi kuti mukwanilitse colinga cina cake . Tingadziŵe bwanji cosankha cimene cidzakondweletsa Yehova ? Cifukwa cakuti timawadziŵa bwino , mwina tingaganize kuti sangakhumudwe ngakhale titakamba nao mosasamala . Peter anali na kabuku kolembamo zocitika za pa umoyo wake . Mulungu angayankhe m’njila imene sitingazindikile . ( Ŵelengani Mateyu 22 : 31 , 32 . ) Kodi muganiza kuti Rehobowamu anamvela bwanji Yehova atamuletsa kumenya nkhondo ? Conco , n’taŵelenga Maliko 10 : 21 limene pali ciitano ca Yesu cakuti , ‘ Bwela ukhale wotsatila wanga , ’ n’nafunitsitsa kukhala Mboni . Wamasalimo anacita zimenezo mwa kuganizila za ubwenzi wake ndi Yehova . ( Sal . Iye wandithandiza , moti mtima wanga ukukondwela . ” Koma woyang’anila dela ananiuza kuti nizayamba kutumikila m’tauni imene n’nabadwila . Ngati mwadwala kwambili , kodi muyenela kuyembekezela kuti Yehova kapena Yesu adzakucilitsani mozizwitsa ? M’kupita kwa nthawi , anthu anakwanitsa kumvetsetsa maulosi a Mulungu olembedwa m’buku la Danieli , koma pa nthawi yoyenelela imene Mulungu anasankha . Ndinam’funsa kuti , ‘ kodi cimeneco cinali chalichi cotani ? ’ Masiku ano , khamu lalikulu limene lili ndi ciyembekezo codzakhala padziko lapansi kwamuyaya likusonkhanitsidwa . ( Salimo 83 : 18 ) Koma mumtima , n’nali kutsutsa kuti : ‘ Bodza , kulibe Mulungu olo kuti am’patse dzina labwanji . Mau amenewa ndi oona cifukwa dzina la Mulungu limapezeka nthawi zokwanila 7,000 m’Baibulo . Yehova anaucha “ mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa ” cifukwa unali kuimila ufulu wake wosankhila anthu cabwino ndi coipa . Tinakangana kwambili cakuti ine n’nathawa panyumba . 3 : 19 ) N’zoonekelatu kuti Yehova saleka mwamsanga kuthandiza anthu amene ayamba kuyenda njila yolakwika . Mwina mudziŵako njila zinanso zimene anthu ena amacitila zacinyengo . Ngakhale n’conco , payenela kuti panatenga nthawi yaitali ndithu kuti Yobu aiŵale mavuto ake . Tifunikanso kupewa kutaila nthawi yaitali pa zosangulutsa . Munakonzekela bwanji kuti mukatumikile ku malo osoŵa ? Kodi tingawathandize bwanji ? Tinakondwela kwambili kuonananso monga banja . ATATE anabadwila ku Graz , m’dziko la Austria mu 1899 . Conco , io anali mnyamata pa Nkhondo Yoyamba ya dziko lonse . Masiku anonso , wocimwa amene walapa afunika kucitapo kanthu kuti acitilidwe cifundo na Mulungu . Anthu masauzande ambili amabatizika caka ciliconse . Ena mwa anthu amenewa ni acicepele . Zoona , nthawi zina timafunikadi kusintha maganizo athu . Yesu anakamba fanizo la wamalonda woyendayenda ndi la cuma cobisika . Kodi mafanizo amenewa amatanthauza ciani ? Kodi pamakhala mapindu anji ngati tilemekeza anthu amene ali pa udindo ? Koma cokondweletsa n’cakuti sanakhalemo mpaka kale - kale . Kodi anthu a Yehova anakhala motani mtundu woyela ? Zingakuthandizeni kuti muzimvetsetsa Malemba . Iye anapezeka kuti akutumikila monga kapolo m’nyumba ya munthu wochuka waciiguputo . Angazidziona kuti ndi acabe - cabe ndi kuti utumiki wao kwa Yehova ndi wopanda phindu . N’cimodzi - modzi ndi mgwilizano wa zipembedzo masiku ano . Kodi timaona uthenga umenewu kukhala wofunika kwambili ? Joy , amene tachula kuciyambi kwa nkhani ino , waona kuti mwamuna wake wasintha kucokela pamene anayamba kuphunzila Baibulo ndi Mboni za Yehova . Ophunzila Baibo oyenelela asanabatizike monga Mboni za Yehova , amafunsiwa mafunso aŵili pa gulu la anthu . NYIMBO : 24 , 99 Usiku tinali kucoka pa cisumbu cina kupita pa cina ndi boti . Kuwonjezela pa kukamba mau olimbikitsa , kodi akulu angalimbikitse bwanji ena ? Sakura lomba ni mpainiya wanthawi zonse , ndipo salinso wosungulumwa . Bwanji ngati mwamuna wanu si Mboni , ndipo muona kuti sakucitilani zinthu mokoma mtima ? Ngakhale kuti Ayuda ndi Akristu anakopa Mau a Mulungu mobwelezabweleza , uthenga wa Mulungu unatetezedwa . Carin atakhalanso ndi mimba , mwamuna wake wosakhulupilila anam’limbikitsa kuti aicotse . Komabe , gulaye inali cida coononga . — Oweruza 20 : 16 . [ Cithunzi papeji 31 ] Cithunzi coonetsa asilikali a Asuri oponya miyala akuukila mzinda wa Ayuda [ Eni ake ] © Erich Lessing / Art Resource , NY Koma , sindinakhulupilile zimene io anandiuza . ” Mosakaikila , alongo olimba mtima amene tinafunsa anakumana na mavuto . Koma akuyembekezela kutha kwa dongosolo loipa lino la zinthu pa “ tsiku la Yehova . ” ( a ) Tingakambitsilane bwanji ndi munthu amene amakhulupilila moto wa helo ? Lugarà ) , 7 / 1 Bamboyo anati : “ Palibe amene adziŵa zimene zimacitika , tingofunika kuyembekezela . ” Pamene n’nali kufunsa Mary mafunso , n’nacita cidwi ndi mmene anali kuonela zinthu zauzimu . Akanakhala kuti anali kuona nchito yomanga kacisi wa Yehova monga yosafunika , sembe sanayende mtunda wautali wa makilomita pafupi - fupi 1,600 , kupitila m’dziko loopsa . ( Maliko 1 : 14 , 15 ) Mopanda mantha , Yesu anadzudzula atsogoleli acipembedzo aciyuda . Ici n’cifukwa cinanso cimene anamuphela . — Maliko 11 : 17 , 18 ; 15 : 1 - 15 . Ngati mwapatsidwa mwayi wotsogoza pa kukumana kokonzekela ulaliki , mungacite zambili pothandiza okalamba kutengamo mbali mu nchito yolalikila . N’ciani cingathandize mwamuna ndi mkazi kukhala ogwilizana ? Nanga ndani amene amagwila nchito yaikulu imeneyi ? Ndipo Lameki anakhala munthu wacikhulupililo colimba . Cifukwa cakuti panthawiyo odzozedwa adzakhala atalandila cidindo cao comaliza . Mlongo wina wa mumpingo wathu , amene mwamuna wake sanali Mboni , anabwela kunyumba kwathu m’mamaŵa na kunipatsa emvulupu . Mwacitsanzo , nthawi ina atakhala kale Mkhristu , abale onse ku Yerusalemu ‘ anali kumuopa , cifukwa sanakhulupilile kuti anali wophunzila . ’ — Mac . Kuwonjezela apo , kuika zofalitsa zathu pa mawebusaiti amene amalola anthu kupeleka ndemanga , kumapatsa ampatuko ndi anthu ena otsutsa mwayi wocititsa anthu ena kuyamba kukayikila gulu la Yehova . Kodi kupatsa kuli na ubwino wanji kwa ife ? Monga Mfumu na Mkulu wa Ansembe , kodi Yesu amagwila nchito yanji ? Ndinali kungoganizila za ine ndekha basi . ( Maliko 1 : 10 - 12 ) Pa utumiki wake wonse wa padziko lapansi , mzimu woyela wa Mulungu unathandiza Yesu kucita zozizwitsa ndi kulankhula ndi ulamulilo waukulu . ( Mac . 20 : 29 , 30 ) Mpatuko wonenedwelatu umenewu unaonekela kwambili pamene atumwi onse anamwalila . — 1 Yoh . Conco , pamene n’nali kutumikila pa Beteli , m’pamene n’nakumana ndi Angela , mlongo wanzelu amene tsopano natumikila naye kwa zaka 58 . ( Onani pikica namba 1 kuciyambi . ) Kukhala na cidziŵitso colongosoka kunathandiza Nowa kukhala na cikhulupililo komanso nzelu yocokela kwa Mulungu . ( Mlal . 12 : 14 ) Yehova popeleka ciweluzo amapenda zinthu zina zimene ife sitingazidziŵe . Nanga n’cifukwa ciani tifunika kusankha kum’konda ? Ndi ciyembekezo cotani cimene odzozedwa ali naco ? Inde , zinamulimbikitsa kucitapo kanthu . Cikondi sicitha . ’ — 1 Akorinto 13 : 4 - 8 . H . Anamuuzanso kuti zikanakhala bwino ngati iye akanakonza cakudya cocepa cabe . Iwo amazindikila mfundo yakuti Yehova ndiye anawamanga pamodzi , ndipo afuna kuti iwo akhale ‘ ophatikana ’ kwa wina ndi mnzake . Anthu akamvela amuna amenewa , m’ceni - ceni anali kutsatila Yehova monga Mtsogoleli wawo . Ndi uthenga wotani umene otsatila a Yesu ayenela kulalikila ? Ubwenzi umatanthauza mmene anthu aŵili amamvelela akamaganizilana ndiponso mmene amacitila zinthu kwa wina ndi mnzake . Nanga anacita ciani kuti azikonzekeletse ? Koma n’cifukwa ciani kuyeletsa n’kofunika kwambili ? ( b ) Kodi pampingo pali makonzedwe otani okhudza kuyeletsa pa Nyumba ya Ufumu ? Molingana na Hana na Samueli , ise Akhristu masiku ano tili na mwayi woseŵenzetsa moyo wathu potumikila Mlengi wathu . Ena mwa anthu amenewa ali ngati nsomba “ zabwino , ” ndipo amasonkhanitsidwila mumpingo wacikristu . Na imwe muyenela kuti pali zimene mumakhulupilila pankhaniyi , malinga ndi kumene munakulila kapena cikhalidwe canu . Mwacitsanzo , pafupifupi maiko 175 anagwilizana zakuti aletse anthu kukoka fodya , ndipo izi zinayenela kucitika podzafika mu August 2012 . Mabuku 66 ouzilidwa amenewa onse pamodzi amapanga Baibo yathunthu — Uthenga wocoka kwa Mulungu kupita kwa anthu . Mofananamo , Mkristu amene wafooka cifukwa ca mavuto aakulu , angafunike nthawi kuti akhalenso wolimba kuuzimu . Pambuyo pa nkhani , anthu oposa 600 anatsalila kuti amvetsele mbali ya mafunso ndi mayankho . Ndipo zimenezi zikhoza kuononga ubwenzi wathu ndi abale athu . N’nayamba kuona mtendele na kusunga cakukhosi monga kum’maŵa na ku m’madzulo . Koma kuyamikila Yehova kuti ndinali kusangalala ndi mkazi wanga , ndiponso kuti ndinali ndi mwai wotumikila Mulungu ndi munthu amene anali kumukonda kwambili , kwandithandiza kuona zinthu moyenela . ” Komabe , ndi anthu ocepa amene anatsatila malangizo amenewa . Kodi kulambila kwa pabanja kumalimbikitsa bwanji mgwilizano ? Komabe , iye sanataye mtima . Tsiku lina anandipempha kuti ndipite naye ku misonkhano . Muzisonyezana kukoma mtima kosatha ndi cifundo . ” — ZEK . Kodi amacita bwanji zimenezi ? TIZIONA ZABWINO MWA ENA Motsogoleledwa ndi Mau a Mulungu , Yosiya anayamba nchito yaikulu yocotsa mafano . Anakonzanso zakuti acite cikondwelelo ca Pasika cimene sicinacitikepo kumbuyoku . Wamasalimo anaimba kuti : “ Yehova ali pafupi ndi anthu a mtima wosweka . Mabwenzi amakhala ndi nthawi yoceza . Malinga ndi zimene Kayla anakamba , mungaonetse kuti ndinu ofikilika mwa kumvetsela modekha kwa mwana wanu . Anthu pafupi - fupi 20 anapezekapo , ndipo ena anali kufunsa mafunso pa zimene Baibo imakamba . Koma anamwali anzelu akukana kuwathandiza . Munthu ukamatumikila mumpingo wa cinenelo cina umakhala monga uli ku dziko lina . Paulo analemba kuti : “ Pamene akutinenela zacipongwe , timadalitsa . Omasulila anali kudzaphunzitsidwa mmene angazimvetsetsela Cingelezi , mmene angakhalile aluso panchito yao , ndiponso mmene angamagwilile nchitoyo mogwilizana . Kodi tiyenela kukonzekela ciani ? Muphunzitseni kuti azitsogoza bwino misonkhano yokonzekela ulaliki . Ena anaphedwa mu ulamulilo wa Nazi ku Germany . Musalole Kuti Cikondi Canu Cizilale , May ( b ) Nanga tiphunzilapo ciani pa zimene Yesu anayankha ? N’cifukwa ciani n’zosavuta Mkhristu kukhala na colinga cofuna - funa nchito yapamwamba ? Ife tonse tili ndi mwai wolengeza uthenga wabwino . Mtumwi Paulo anali kucitila cifundo ngakhale anthu amene anali kum’tsutsa mwaciwawa . Caka cotsatila , ife tonse atatu tinadzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa . Mfundo zonsezi zinalembedwa kaamba ka ubwino wathu . — Aroma 15 : 4 . Mwacitsanzo , nthawi ina mtumwi Yakobo anapatsa uphungu abale ake cifukwa anali kukondela anthu olemela . Muziseŵenzetsa zida zothandiza pophunzila Baibo . N’ciani cingatithandize kuti tisalole mkwiyo kutilamulila ? Koma Yehova anasungila mwana wake waumunthu woyamba , mwayi wopatsa zinyama maina . Njila imodzi imene makolo angacitile zimenezi ni mwa kukhala na pulogalamu yokhazikika ya Kulambila kwa Pabanja . N’ciani cingaike umoyo wathu wauzimu paciswe ? Iye anamva ‘ phokoso la mafupa kuti gobedegobede , ndipo pa nthawiyo mafupawo anali kubwela pamodzi n’kumalumikizana . ’ Baibulo limatiuza kuti Yehova Mulungu “ sakhala mu akacisi opangidwa ndi manja . Mofananamo , tidziŵa kuti nchito yopanga ophunzila yapita patsogolo kwambili . Koma “ cilango ” cimaphatikizapo mbali zingapo . Yelekezelani kuti mukuona mnyamatayu atavala covala cacifumu , akupita m’maudzu aatali , akukwela m’phili ndipo akupita m’chile mmene muli minga kufunafuna nkhosa yotayika . Kodi taphunzila ciani pa zimene takambilana zokhudza mafumu anayi aciyuda amene anatumikila Yehova ndi mtima wathunthu ? Zili conco cifukwa cakuti ndife opanda ungwilo , ndipo ‘ mtima wathu ndi wonyenga kwambili kuposa cina ciliconse ndipo ungathe kucita cina ciliconse coipa . ’ ( Yer . 3 : 17 ; 13 : 10 ; 17 : 9 ; 1 Maf . Pamene Yesu anabwela padziko lapansi , Aisiraeli anapitilizabe kusamvela Yehova ndi aneneli ake cakuti Yesu anacha Yerusalemu kuti “ wakupha aneneli . ” Mwacitsanzo , wapatsa Mwana wake udindo woyang’anila mpingo , ndipo Mwanayo anasankha “ mtumiki woyang’anila nyumba wokhulupilika ” kuti azipeleka cakudya cauzimu pa nthawi yoyenela . A Yohane : Iyi , yakuti “ Cikwati Ndi Mphatso Yocokela kwa Mulungu Wacikondi . ” Monga mmene zinalili kwa ine , panafunika nthawi kuti azindikile kuti zimene anali kukhulupilila zinali zabodza . Akatswili opanga miseu aciroma anapanga miseu yosiyanasiyana ndipo yonse pamodzi inakwana makilomita 80,000 . Poganiza kuti nabwela kudzalandila thandizo lakuthupi , ananifunsa kuti , “ N’ciani cavuta ? ” Ndi kamvedwe kotani kamene tili nako masiku ano ? Abulahamu anafuna kukhalabe pamtendele ndi Loti , conco anam’patsa mwai wosankha malo abwino . Atamuuza za banja lake , mwamunayo anakondwela kwambili . Ciyembekezo camphamvu n’cofunika kwambili kuti tipilile cizunzo . Tikaonetsa munthu wogontha vidiyo ya citundu ca manja , amacita cidwi kwambili . ( b ) Tiphunzilapo ciani pa zimene zinacitikila Eliya ? Anakamba kuti Ahabu , mkazi wake , ndi ana ake adzaphedwa mmene iwo anaphela Naboti ndi ana ake . — 1 Maf . Tingacite ciani kuti zolakwa za ena zisatipangitse kuwononga ubwenzi wathu na Yehova ? Mu 1960 , anatipempha kukatumikila ku ofesi ya nthambi ya ku Puerto Rico . Ofesiyi inali nyumba ing’ono yasanjika mumzinda wa Santurce , San Juan . Cifundo cimene Mulungu anaonetsa m’zitsanzo za m’Baibo zimene takambilana m’mapalagilafu apitawa , cinali coyenelela . Popeza dziko lathu lapansi si paradaiso masiku ano , kodi tingatsimikize bwanji kuti lonjezo limeneli lidzakwanilitsidwa ? Malinga ndi zimene ofufuza ena anapeza , anthu pafupi - fupi 60 miliyoni anafa pa Nkhondo Yaciŵili ya Padziko Lonse . Tifunika kutengelapo phunzilo pamenepa , cifukwa tikukhala m’nthawi imene anthu ambili alibe cikhulupililo na ciyembekezo . Izi zili conco cifukwa cakuti ena akambapo kuti “ cifundo na kukoma mtima zimathandiza munthu kuti asamakwiye - kwiye kapena kukhumudwa . ” MBILI YANGA : KATSWILI WOPONYA ZIBAKELA Nditalowa , nkhani ya anthu onse inali pafupi kutha . Motelo , ndinaganiza kuti ndimvetsele nao phunzilo la Nsanja ya Mlonda . Nthawi zonse tinali kucita phunzilo la banja lotsatilika , ndipo tinali kuyelekezela zinthu zimene zingacitike kusukulu . Ganizilani cabe , kukhala m’dziko imene palibe akudwala matenda a mtima , khansa , maleliya , kapena matenda ena alionse . Amuna ake , a Pranas , anakamba kuti ana ao anali kudzipeleka nthawi zonse kuthandiza ena pa misonkhano ikuluikulu . Nayenso M’bale Fred Twarosh anati : “ Onse pamsonkhanowo anaimilila panthawi imodzi . ” Ingakuthandizeni pa umoyo wanu tsopano . Onse amene akhulupilila Yesu adzakhala na moyo wamuyaya . Moyo umenewo udzatheka cifukwa ca nsembe ya Yesu , yochedwa “ dipo . ” — Aroma 3 : 24 . Nthawi zambili sitingafunikile kugwilitsila nchito masitepe onse atatu amene ali pa Mateyu 18 : 15 - 17 . Ngati n’conco , muli ndi colinga cabwino . Ndi zabwino komanso zosangalatsa kwambili Abale akakhala pamodzi mogwilizana ! ” — Sal . Koma n’cifukwa ciani Yesu anali kucita zozizwitsa ? Atafika zaka 18 , manja ake anakhalanso bwino . Kenako anapita ku yuniveziti . Kodi Yesu anapeleka malangizo anji ponena za ndalama ? Kodi n’ziti zingakhale zifukwa zomveka zopatukilana ? Amuna amenewa amacita mbali yofunika kwambili pa nchito yosamalila anthu a Mulungu . Zocitika zofanana ndi zimenezi zinacitikanso ku Argentina ( Yearbook ya 2001 , tsamba 186 ) ; East Germany ( Yearbook ya 1999 , tsamba 83 ) ; Papua New Guinea ( Yearbook ya 2005 , tsamba 63 ) ; ndi Robinson Crusoe Island ( Nsanja ya Olonda ya June 15 , 2000 , tsamba 9 ) . Macaputala aŵiliwa ndi ogwilizana kwambili , koma caputala ciliconse cikufotokoza zinthu zimene sizinachulidwe m’caputala cina . 4 : 12 ; Yak . Ngakhale kuti zinthu n’zovuta kuno , anthu akulandila uthenga wabwino , ndipo ndikuwathandiza kuyandikila kwa Yehova . Sembe Ababulo anadziŵa mapulani a Koresi , sembe anatseka mageti onse amene anali otseguka . Kodi ciyembekezo cingakhale bwanji ngati nangula ? PAMENE Yesu anali kuphunzitsa ophunzila ake kulalikila uthenga wabwino , anadziŵa kuti si anthu onse amene adzalabadila uthengawo . Kodi sudziŵa kuti uli ndi moyo cifukwa ca io ? Anthu afunika kudziŵa kuti dipo ni njila yacikondi imene Yehova anapeleka ku mtundu wa anthu kuti akhale ndi ciyembekezo ca moyo wa muyaya . 15 : 58 . Iwo amaonanso kuti ngakhale kuti Mboni zina ndi zosauka , nthawi zonse zimavala ndi kuoneka bwino kuposa anthu ena . ” Nchito yokama mkaka ku ng’ombe ndi kudyesela nkhumba ndi nkhuku inali yosiyana ndi nchito yanga yovina . Timakumbukila kuti m’bale kapena mlongo ameneyo nayenso amatumikila “ Mulungu amene amapatsa mtendele . ” — Aroma 15 : 33 ; 16 : 20 . Posakhalitsa , iwo anayamba kucititsa maphunzilo a Baibo okwanila 23 . 7 : 1 ) Ndi maso a cikhulupililo , kodi mumaona angelo amenewo kuti atsala pang’ono kusiya kugwila mphepo zoononga za cisautso cacikulu padziko lapansi ? Mwacitsanzo , m’Baibulo lina , Uthenga Wabwino wa Maliko , unali utagaŵidwa m’macaputala 50 osati 16 amene alipo masiku ano . N’nayamba kupepa fwaka ndipo posapita nthawi , cinakhala cizoloŵezi canga . Cikondi cimaphatikizaponso kukomela mtima ena , kuwadela nkhawa , ndi kukhala nawo paubwenzi . Imfa , Mdani Wotsilizila , Idzaonongedwa , 9 / 15 3 : 13 ) Koma kodi zimenezi zingatheke bwanji popeza tonsefe ndife opanda ungwilo , timacimwa ndi kufa cifukwa ca kusamvela kwa Adamu ? Koma zitanthauza kuti mkazi akakhala ndi ana amakhala wotangwanika kusamalila anawo ndi kugwila nchito zina za pakhomo , ndipo izi zingam’thandize kupewa mijedo na kuloŵelela m’nkhani za eni . ( 1 Tim . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana zimene amuna ndi akazi angacite kuti ateteze cikwati cao ku ciwelewele . Zingakhale zothandiza kuŵelenga Baibulo kuti tidziŵe okana Kristu amenewa , ndipo mauwa amapezekamo nthawi zokwanila 5 . Mkristu wa Mboni za Yehova wobatizidwa amacotsedwa mumpingo ngati anacita chimo lalikulu ndipo sanalape . Kodi tiphunzilapo ciani pa zimene Yehova anacita pofuna kuthandiza Aisiraeli ocimwa kuti alape ? Iye anali wokonzeka kucita ciliconse cimene anauzidwa monga mmene kapolo amacitila . Cocitika cimeneci ndi cimodzi mwa zocitika zosangalatsa kwambili ndiponso cosaiŵalika . ” Tifunika kucitila ena cifundo maka - maka cifukwa cofuna kutengela Yehova Mulungu ndi kum’lemekeza monga Gwelo la cikondi na cifundo . ( Miy . Atafika zaka 19 , Vitaly , anapita kukacita upainiya wapadela . Mphunzitsi wina dzina lake Timothy Evans anati : “ Ana amafunika kulimbikitsiwa monga mmene zomela zimafunikila madzi . Munthuyo anauza Yesu kuti : “ Mukandikumbukile mukakaloŵa mu ufumu wanu . ” Anthu ambili a ku Japan anamvapo mau akuti “ pacipata copapatiza , ” “ kuponyela nkhumba ngale , ” ndi akuti “ musamade nkhawa za tsiku lotsatila . ” ( Mat . Conco , tingacite bwino kudzifunsa kuti : ‘ Kodi napita patsogolo mwauzimu kucokela pamene n’nabatizika ? Nkhondo imeneyo itatha , maufumu ena amphamvu anathelatu . Ubatizo waconco ndiwo wokha wovomelezeka pamaso pa Mulungu . Kodi mukali nato tumapepa twa ciitano twa caka cino tumene mungagaŵile tisanacite Cikumbutso ? Mulimonse mmene zingakhalile , Yesu anaonetsa kuti aliyense ayenela kusankha yekha . Nthawi zambili amishonale amatsogolela mpingo mpaka pamene abale akumeneko akhala oyenelela kutsogolela mpingo . Zinali conco cifukwa Mabaibo anali kucita kuwakopa pa manja , ndipo panali kuloŵa ndalama zambili kuti alembe Baibo . 99 ) Ndipo cinali cokhaulitsadi . 4 : 20 - 24 ; 1 Pet . ( Salimo 139 : 23 , 24 ; Yakobo 4 : 8 ) Ndiye cifukwa cake Yesu analimbikitsa otsatila ake kupemphela , ngakhale kuti Atate ake amadziŵa zosoŵa zathu . Munthu amapanga lonjezo mwa kufuna kwake . N’cifukwa ninji tikamba conco ? Tiziyamikila Kukoma Mtima Kwakukulu Kumene Tinalandila , July 15 : 1 - 6 ; 18 : 9 - 17 ; 2 Mbiri 26 : 16 - 21 ; Dan . Iye anakambanso kuti : “ Ambili a io akali ndi moyo mpaka lelo , koma ena anagona mu imfa . ” Iye analalikidwa mwacindunji na Yesu Khristu , amene anali ataukitsidwa ndi kupatsidwa ulemelelo . ( Luka 19 : 37 - 40 ) Koma Yehova watipatsa mwai wokhala “ anchito anzake . ” Nili na mkazi wanga , Janette ( Deut . 24 : 1 ) Ngakhale kuti ‘ vuto linalakelo ’ sanalichule , mwacionekele silinaphatikizepo zolakwa zing’ono - zing’ono . — Lev . M’malo mwake , iye amayesetsa kuwakondweletsa , ndi kukhulupilila kuti cikondi cao pa Yehova cidzawasonkhezela kum’tumikila mmene angathele . — Mat . Kuti Adamu ndi Hava alandile madalitso amene anawakonzela , anayenela kumvela Yehova ndi kuvomeleza ulamulilo wake . ( Gen . Baibulo limatiuza kuti sitiyenela kukonda zinthu za m’dzikoli . OFESI YA NTHAMBI : Anaika mtima wake wonse pa kucita maphunzilo apamwamba kuti akapeze nchito yabwino ndi kukhala na umoyo wapamwamba . Zithunzi zimenezi zimandikumbutsa kuti umoyo wanga wakhala wopindulitsa . 3 : 8 ; Deut . 4 : 11 ) Kuposa zonse , Yehova amatisamalila mwa kuuzimu . IFE Mboni za Yehova timalikonda kwambili Baibulo . Iye anakhumudwanso pamene anzake a kusukulu anali kumunyoza . “ Odala ndi anthu amene amabweletsa mtendele , cifukwa adzachedwa ana a Mulungu . ” 6 Kodi Angelo Oipa Alikodi ? Ndipo ambili amakhumudwa cifukwa cogwilitsidwa mwala . Koma nthawi zonse Yehova anali kundithandiza kuzindikila kuti ndidzapindula kwambili ndikapitiliza kutumikila . ” Kodi mlongo wina anapindula bwanji atathandiziwa mwacikondi na akulu ? Conco , tingafunse kuti : Nanga mnzathu amene tiyenela kukonda ndani kwenikweni ? Mwacionekele iye adzayankha kuti iyai . Kodi Mboni za Yehova Zimakhulupilila Ciani ? Koma anacitanso zinthu mwanzelu mwa kukamba mokoma mtima ndi Davide . N’cifukwa ciani tiyenela kuyembekezela kuti zinthu padzikoli zidzaipa kwambili pamene mapeto akuyandikila ? N’cifukwa ciani anthu ambili safuna kugwila nchito mwamphamvu ? Ngati mukuvutikabe ndi nkhawa ngakhale pambuyo pakuti mwayesayesa njila zosiyanasiyana , mungacite bwino kukaonana ndi dokotala . Tuakacisi twina tumapangidwa kuti azikumbukilapo nkhondo zochuka , anthu amene anafa pankhondo , kapena pa ngozi zina zacilengedwe . Zinthu zonsezi sizidzawonongedwa . Kapena kodi ndine wakufa ku ucimo ? Ndiyeno , ndinafunika kupanga cosankha cacikulu paumoyo wanga . Kodi ningathawe monga mmene Yosefe anacitila , kapena ningagonje ngati Davide ? ’ Abale amene anali kutsogolela m’mipingo anaona kuti Timoteyo akupita patsogolo . Nthawi zina , amanifunsa mafunso kuti adziŵe zambili . Mwacitsanzo , Paulo analemba kuti : “ Dema wandisiya cifukwa cokonda zinthu za m’nthawi ino . ” 7 : 6 ; Mac . 23 : 8 ) M’malo mwake , anachula za ciukililo ca kumwamba kuti ophunzila ake oona mtima apindule . Ophunzila ake amenewa anali kudzalandila ciukililo cimeneci mtsogolo . Gulu la Yehova lapeleka zida zambili zofufuzila nkhani . Atafika zaka 20 , anapita ku Quebec ku Canada , kumene apainiya anali ocepa kwambili . N’cifukwa ciani ophunzila a Khristu sanafunike kusala anthu a mitundu ina ? Izi zacititsa kuti atsogoleli ambili a zipembedzo alemele kwambili . — Chivumbulutso 17 : 4 , 5 . “ Njoka yakale ija , ” Satana Mdyelekezi , inanyenga Hava pom’pangitsa kukhulupilila kuti kudya cipatso ca “ mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa ” kudzam’patsa nzelu zapadela , cakuti azitha kudzigamulila yekha cabwino ndi coipa . ( b ) Mukufunitsitsa kudzacita ciani pamene Mulungu adzakwanilitsa malonjezo ake ? Ngakhale simukumuona panopa , mumakhulupilila mwa iye . ” Mukanakhala kuti mudzilamulila mwekha ndipo muli na moyo wosatha , kodi muganiza kuti mukanakhala na umoyo wacimwemwe ? ( Yoh . 17 : 11 ) Popeza Yehova ni woyela , mfundo zonse na malamulo ake onse ndi zoyela . 10 : 14 ; Chiv . 4 : 11 ) Popeza kuti Yehova ndiye anatilenga , tonse ndise anthu ake . Kuganizila zinthu zimene sizinaticikilepo kungatithandizenso kutsanzila nzelu za Yehova ndi kudziŵa zotulukapo za zocita zathu . Nanga kuukitsidwa kwake kuli ndi tanthauzo lotani kwa ife ? Mfumu yamuyaya . ” — CHIV . Koma usiku wina , Davide ndi anthu ake anapeza malo amene Sauli ndi asilikali ake anamangapo msasa . Ngakhale kuti Mfumu Sobhuza inalamulila zaka zambili conco , pali mfumu ina imene ulamulilo wake sudzatha cifukwa cakuti iyo sidzafa . Timayamikila kwambili kuti Yehova kupitila mwa abale okhulupilika , anatithandiza ndi kutilimbikitsa mwauzimu . Pamene anthuwo anafunsa Petulo zimene ayenela kucita , iye anawayankha kuti : “ Lapani , ndipo aliyense wa inu abatizidwe m’dzina la Yesu Kristu kuti macimo anu akhululukidwe . Mukatelo mudzalandila mphatso yaulele ya mzimu woyela . ” ( Mac . Ndipo Mose anacitadi zimenezo . ( Eks . Pambuyo powauza fanizo la kapolo wokhulupilika ndi wanzelu , la anamwali 10 , ndi la matalente , Yesu anakambanso za nthawi imene “ Mwana wa munthu ” adzaweluza “ mitundu yonse ya anthu . ” Kumbukilani kuti nthawi ina , Yohane Mbatizi anafunsa Yesu kuti : “ Kodi Mesiya amene tikumuyembekezela uja ndinu kapena tiyembekezele wina ? ” ( Mat . ( Ŵelengani Yeremiya 29 : 11 . ) 4 : 8 ; 5 : 23 ; Aheb . Mulungu adzapatsa Yesu mphamvu zoononga Satana . Cimeneci ni cifukwa cabwino cokhalila ‘ okondwela , na kudumpha ndi cimwemwe . ’ ( Sal . Kodi Akristu acikulile angawaphunzitse ciani acinyamata ? Conco , “ cifukwa ca ucimo wa munthu mmodziyo imfa inalamulila monga mfumu . ” 8 “ Mtendele wa Mulungu . . . N’ciani cimene tinganene ponena za mau acikondi amene ali m’Nyimbo ya Solomo ? M’mbili yonse ya dziko lapansi , makhalidwe sanalowepo pansi monga mmene zilili masiku ano . Ndipo m’caka cimodzimodzico , ndinadzipenyela ndekha wina akuphedwa cifukwa ca mikangano ya pabanja . Nili ndi cikumbumtima cabwino pamaso pa Yehova . Hosi yoyamba ni yoyela , ndipo wokwelapo wake ni mfumu yoikidwa catsopano yaulemelelo . Mneneli Yesaya anakhalapo ndi moyo panthawi zovuta kwambili m’mbili ya Isiraeli . Iye anawauza kuti : “ Inu mumacedwa kumvetsa zinthu . ” N’zoona kuti panthawi ina Mulungu anacilitsa anthu . Mose anawauza kuti : “ Ndi cakudya cimene Yehova wakupatsani . ” Enanso amakwanitsa kulalikila kunyumba ndi nyumba , koma salalikila uthenga wabwino wa Ufumu . Koma Davide anamuyankha kuti : “ Tsopano ndacita ciani ? Tinadabwa kwambili . M’mudzi umodzi cabe umenewo tinapezamo anthu 8 amene sakumva . N’cifukwa ciani munthu angaseŵenzetse malangizo akale - kale amenewo pamene kuli cidziŵitso cambili - mbili ca panthawi yake m’dziko lamakono ? Pambuyo pake , ine n’naikambanso mwacidule m’citundu ca Citagalogi . * Yesu sanasankhe atumwi ake kuti azingoyenda nawo mu ulaliki , koma kuti asenze maudindo aakulu pakati pa anthu a Mulungu . ( Ŵelengani 1 Akorinto 15 : 24 - 28 . ) * Kuyenda pa sitima yaconco kungapangitse kuti ticite ngozi . Atatsiliza maphunzilo , anam’tumiza ku Chile monga mmishonale kumene anakatumikilanso monga woyang’anila dela . Magazi anali kugwilitsidwa nchito kokha pa zocitika zapadela . Conco , molingana ndi ife anthu iwo angathe kusankha kucita zabwino kapena zoipa . Ngati n’conco , kodi vuto lingakhale cizoloŵezi canga cophunzila ? ’ Ngakhale kuti m’baleyo anali ndi nkhawa ponena za kumene adzapeza malo okhala ndi banja lake , iye anati : “ Yehova adzatithandiza kupeza malo ena . Lemba la Levitiko 12 : 6 limati : “ Ndiyeno masiku a kuyeletsedwa kwake cifukwa cobeleka mwana wamwamuna kapena wamkazi akakwana , azibweletsa kwa wansembe , pakhomo la cihema cokumanako , nkhosa yaing’ono yamphongo yosapitilila caka cimodzi kuti ikhale nsembe yopseleza . Ndipo tonse timalemekeza malamulo a cilengedwe . M’magaziniyo munalinso cithunzi coonetsa abale ali m’miseu ku Mexico City . Mau ake amati : “ Ndimanena za mapeto kuyambila pa ciyambi . Kuyambila kalekale , ndimanena za zinthu zimene sizinacitike . ” Angaone duŵalo kukhala lapadela poyelekezela na maluŵa ena onse pa nyumbapo . Kuyankha Mafunso a M’Baibo 32 Tinadziŵa kuti tidzaluza mlanduwo , koma tinazindikila kuti udzakhala mwayi wathu wocitila umboni . “ Munthu wacikulile uzim’patsa ulemu . ” — LEV . Tinapeza malo abwino osonkhanilapo na kuwakonza . 4 : 6 , 7 ) Nthawi zonse tifunika kukhala oyamikila cifukwa ca “ mtendele wa Mulungu ” umene ndi wapadela ndipo umateteza mitima yathu ndi maganizo athu . 6 : 4 . Yehova atayamba kulenga zinthu , mwacikondi anasankha kupatsa zolengedwa zake zaluntha ufulu wosankha zocita . N’ciani cinawalimbikitsa kusamukila ku maiko acilendo ? Ndipo Zera Mwitiyopiya ndi gulu lankhondo la asilikali 1 miliyoni ndi magaleta 300 wabwela kudzamenyana ndi Yuda . Kodi anthu amene amatsatila mfundo za m’Baibulo amaonedwa bwanji ? A Inoki : Palibe vuto . Tingathandize bwanji kukongoletsa paladaiso wauzimu ? 20 : 1 , 2 . Komabe , tingafunse kuti , kodi zimenezi zidzacitika liti ? Rehobowamu analidi wosiyana kwambili na Mfumu Davide , ambuye ake ! Ngati timakonda Mulungu , kodi tiyenela kucita zotani ? Thandizo limene limapelekedwa kwa magulu omasulila mabuku padziko lonse , limaonetsa kuti gulu la Yehova limaona nchito yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu padziko lonse kukhala yofunika kwambili . ( b ) Kodi zosankha zimene tinapanga kale tifunika kuziona bwanji ? Ndiye mungam’funse kuti : “ Ngati lesipi ya keke inalembewa na winawake , nanga n’ndani analemba lesipi yovuta kuimvetsetsa ya apozi ? ” ( Machitidwe 20 : 35 ) Tikamagwila nchito , pali anthu amene amapindula monga makasitomala ndiponso anthu amene anatilemba nchito . 12 , 13 . ( a ) Kodi cikwati ca Mwanawankhosa cidzacitika liti ? Mu 1981 , tinakumananso ndi gulu lina landale la acinyamata . Komabe , n’kutheka kuti ena mwa mbadwa za Efuraimu anathaŵila m’dela la Yuda . Kodi mboni ziŵili ndani ? Komanso anali kucita zinthu mogwilizana na cifunilo ca Mulungu na miyezo yake . ( Yoh . Coyamba , Yesu anadzozedwa mwacindunji ndi Yehova . “ Pakuti kukonda ndalama ndi muzu wa zopweteka za mtundu uliwonse , ndipo pokulitsa cikondi cimeneci , ena asoceletsedwa n’kusiya cikhulupililo ndipo adzibweletsela zopweteka zambili pathupi lawo . ” — 1 Timoteyo 6 : 10 . Kuonjezela pamenepo , gululi linalipo pamene Yohane anali kulemba kalata yake mu “ nthawi yakumapeto , ” pamene atumwi anali kutha . Tonse timasangalala kulandila cilimbikitso pa misonkhano yathu . 24 : 45 ) ‘ Kapoloyu ’ amaseŵenzetsa kokha mawebusaiti ake ovomelezeka pogaŵila cakudya cauzimu . Mawebusaiti amenewa ni www.jw.org , ttv.jw.org , na wol.jw.org . 9 : 36 - 41 ) Mulungu sanaiŵale zinthu zabwino zimene Dorika anacita . Koma mwina mungafunse kuti , ‘ N’cifukwa ciani ena amaopa kuceleza anzawo ? ’ Kumapeto kwa moyo wao , Bezaleli ndi Oholiabu sanalandile mendulo , cikho , kapena zinthu zina powayamikila kaamba ka zinthu zimene anapanga ndi kumanga mwaluso . Mosakaikila , anthu a m’zipembedzo zonse komanso anthu amene sali m’cipembedzo amaonetsa kukoma mtima kumeneku . Masiku ano , n’zosavuta kuganiza kuti anthu oipa samalangidwa . Baibo imati : “ Moyo [ wa munthu ] sucokela m’zinthu zimene ali nazo . ” Tidziŵa zimenezi cifukwa mouzilidwa ndi Yehova , Davide anapemphelela zinthu zimenezo . Akhristu amene akukila m’dela lanu kucokela ku maiko ena angayamikile kuwauzako zovala zoyenelela zimene angavale m’nyengo yotentha , yozizila , kapena yamvula . Ndi mbali iti imene inali yofunika kwambili kwa Yesu pophunzitsa ? ( Yesaya 35 : 6 ) Ngakhale kuti nthawi zina amakhumudwa , iye amasangalala . Pofotokoza cimene analembela kalatayo , Petulo anati : “ Ndakulembelani zimenezi kuti ndikulimbikitseni ndi kupeleka umboni wamphamvu wakuti kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu n’kumeneku , ndipo mukugwile mwamphamvu . ” 9 : 26 , 27 ) Kodi tingadziŵe bwanji ngati tili ndi mtima wodzikonda ? Apa ndi pamene maulosi ena amene timaŵelenga m’buku la Danieli anali kudzakwanilitsidwa . Nayenso Elizabeth Fot , mtumiki wokhulupilika wa Yehova anali kukhala ku Kant . Kumiko ( pakati ) Mitundu yonse ya anthu idzasonkhanitsidwa kwa iye ndipo adzalekanitsa anthu , mmene m’busa amalekanitsila nkhosa ndi mbuzi . Conco , wothaŵayo sanali kukhala mwamantha poopa kuti mwina adzaphedwa na wobwezela magazi . Tingacite ciani kuti tizipindula kwambili pophunzila Baibulo ? Ndipo nthawi zina , n’zosatheka kusintha zimene tinalakwitsa . Anakamba kuti Mulungu “ amapatsa anthu onse moyo , mpweya , ndi zinthu zonse , ” ndipo “ cifukwa ca iye tili ndi moyo , timayenda ndipo tilipo . ” “ Yehova akapanda kulondela mzinda , alonda amakhala maso pacabe . ” — SAL . 127 : 1b . Vomelezani kuti inunso munacititsa kuti pakhale vutolo , ndipo pepesani mocokela pansi pamtima . Iye anawauzanso kuti : “ Mwakutelo , onse adzadziŵa kuti ndinu ophunzila anga , ngati mukukondana . ” Yankho ili mu salimo limodzi - modzi mmene iye anafunsa kanayi konse kuti : “ Kufikila liti ? ” ( 2 Petulo 3 : 10 - 12 ) Malinga ndi mmene nkhaniyi ikuonetsela , “ zinthu zonsezi ” zimene zidzasungunuka zikuphatikizapo olamulila a dziko loipali ndiponso anthu amene amasankha ulamulilowo m’malo mwa ulamulilo wa Mulungu . Ena amene anali aneneli aakazi ndi Miriamu , Hulida ndi mkazi wa Yesaya . — Ekisodo 15 : 20 ; 2 Mafumu 22 : 14 ; Yesaya 8 : 3 . ( Mat . 28 : 18 - 20 ) Popeza Yesu ni colengedwa cauzimu cosaoneka kumwamba , kodi akanatsogolela bwanji anthu a Mulungu padziko lapansi ? Limati : “ Popeza zinthu zonsezi zidzasungunuka , ganizilani za mtundu wa munthu amene muyenela kukhala . Muyenela kukhala anthu akhalidwe loyela ndipo muzicita nchito zosonyeza kuti ndinu odzipeleka kwa Mulungu . Komanso nimakondwela poona kuti adzukulu anga nawonso akuphunzila za Mulungu . Ni mapindu anji amene tingapeze ngati tipitiliza kukhala na khalidwe labwino ? Ganizilaninso za Mkazi wamasiye wosauka wa m’nthawi ya Yesu . Zimenezi zidzatithandiza kuonjezela ndi kulimbitsa cikhulupililo cathu . Cifukwa ca imfa ya Yesu , machimo athu amakhululukidwa ndipo timakhala ndi ciyembekezo ca moyo wamuyaya . Kuyambila panthawiyo , pa Cinai paliponse m’maŵa tinali kuphunzila mitu itatu . Iye anali woolowa manja ndipo anapeleka malipilo ofanana kwa anchito onse , kaya anaseŵenza tsiku lonse kapena ola limodzi cabe . Anthu ambili amaganiza kuti ndi bwino kungotsatila zimene mtima ufuna posankha zocita . Kodi inu simumaziona zimenezi ? ( b ) Fotokozani mmene Adamu anaseŵenzetsela ufulu wake wocita zinthu . Nanga bwanji za kufatsa , mtendele , na cikondi ? Monga mmene zinalili m’nthawi ya atumwi , masiku anonso mumpingo wacikhristu mulibe akulu angwilo , pakuti “ tonsefe timapunthwa nthawi zambili . ” Zimenezi zinatheka pamene Yesu anabwela padziko lapansi ndi kupeleka moyo wake monga nsembe . Anthu ena anaona kuti kalendala ya Mayan imene inatha pa December 21 , 2012 inali ndi cenjezo la zocitika zoopsa . Iwo ndiwo adzakhala “ Yerusalemu watsopano , ” mkwatibwi wa Khiristu . ( Chiv . 4 : 10 ) Koma mu 1932 , patangopita zaka zisanu , akopotala 103 ndi ofalitsa ena ku Japan anagwila nchito yolalikila , ndipo anagaŵila mabuku oposa 14,000 . Mwacitsanzo , pamene kuipa kunaculuka kwambili m’mizinda yakale ya Sodomu ndi Gomora , Mulungu anauza Abulahamu kuti : “ Ndiye nditsikilako kuti ndikaone ngati akucitadi monga mwa kudandaula kumene ndamva ndiponso ngati zocita zao zilidi zoipa conco . Kuthandiza Alendo Ocokela ku Mayiko Ena “ Kutumikila Yehova Mokondwela , ” May Ni zopinga ziti zimene zingatilepheletse kuceleza ena ? Amaphuka ngati duwa n’kuthotholedwa . Yehova amanyansidwa ndi kupeleka anthu nsembe . N’zoona kuti timalandila madalitso ambili cifukwa ca kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova . Tiyeni tione zitsanzo za m’Baibulo za anthu amene anaona dzanja la Mulungu ndi za amene sanalione . Lemba la Deuteronomo 24 : 14 , 15 limati : “ Usacitile cinyengo waganyu wovutika ndiponso wosauka n’kumubela , kaya akhale mmodzi wa abale ako kapena mmodzi mwa alendo okhala m’dziko lanu . . . Ngakhale masiku ano , mwacizoloŵezi anthu amachula malo okongola kwambili kuti paradaiso . ( Luka 12 : 54 - 56 ) Mosiyana na nzelu zacibadwa za dokowe , kudziŵa Mulungu ndi kumene kumathandiza anthu kuzindikila tanthauzo la zinthu zimene zicitika masiku ano . Jairo anali kukhumudwa kwambili akaona kuti anthu sakumvetsa zimene anali kukamba . Nkhani youzilidwa imeneyi imakamba kuti Mose “ anacha malowo Masa ndi Meriba , cifukwa ana a Isiraeli anakangana ndi Mose , komanso cifukwa ca kuyesa Yehova kuti : ‘ Kodi pakati pathu pano , Yehova alipo kapena ayi ? ’ ” ( Eks . Kodi magulu a nkhondo amenewa adzaphatikizapo anthu ena ? Komabe , mu December 1952 , boma linaniitana kuti niloŵe usilikali . Kodi angelo anathandiza bwanji Yoswa ndi Hezekiya ? Kwanicititsanso kuti nizikwanitsa kukhala bwino na abale a zikhalidwe zosiyana - siyana . ” 3 : 15 ) Komanso Mose “ anayang’anitsitsa pamphoto imene adzalandile , ” ndipo zimenezi zinamuthandiza kusonyeza cikhulupililo ndi kukulitsa cikondi cake pa Yehova . ( Aheb . Pemphelo lina la Solomo linaonetsa kuti Yehova anayanja anthu amene sanali Aisiraeli . Vuto limeneli ni imfa ya mnzawo wa m’cikwati . Ingakuthandizeni kudziŵa mmene 5 : 8 ; Chiv . 12 : 17 ) Conco , n’zosadabwitsa kuti nthawi zina , ngakhale ise atumiki a Mulungu timakhala na nkhawa . M’kupita kwa zaka , Davide anamwalila ali wokhulupilika , ndipo mbili ya cikhulupililo cake inasindikizika m’cikumbukilo ca Yehova . — Aheb . “ Ndinali kukayikila ngati Mulungu amatisamaliladi . Timoteyo anafunikila kudziŵa zimenezi . Nanga tingacite ciani kuti tiupewe ? Cifukwa ca mantha , iwo anangoponya mtembowo m’manda a Elisa n’kuthaŵa . Mukatelo , mudzasonyeza kuti muli ndi maganizo monga a Davide amene anati : “ Yehova , ine ndimakonda nyumba imene inu mumakhala . ” — Salimo 26 : 8 . Pamene Daniel ndi anzake anatengedwa ukapolo , Ababulo anayesa kuwasintha kuti agwilizane na cikhalidwe cawo mwa kuwaphunzitsa “ cinenelo ca Akasidi . ” Zinthu zimenezo zingakhale msampha , ndipo zingatilepheletse kucita zinthu zakuuzimu monga kuphunzila Baibulo , kukonzekela ndi kupezeka pa misonkhano , ndi kupita mu ulaliki nthawi zonse . ( b ) N’ciani cinali kufunikila kuti Isiraeli wa kuuzimu akalamulile ndi Kristu kumwamba ? ( 1 Akorinto 8 : 11 , 12 ) Kapenanso cikumbumtima cathu ndiye cosaphunzitsidwa bwino . Kaŵilikaŵili tinali kuganiza kuti mwina sitinamulele bwino mwanayo . ” Cosankha cabwino cimene Carin anapanga poyamba cinam’thandiza kupanganso cosankha cimene cinasangalatsa Yehova . Onse aŵili anayamba kuvutika , kenako anafa alibe ciyembekezo ciliconse . Tikacita zimenezi , sizidzativuta kumvela Yehova ndi kukhala naye pa ubwenzi . — 1 Yohane 2 : 15 - 17 . Koma patapita zaka 6 , banjali linakumana na vuto . Viŵanda vimadziŵa kuti Mulungu aliko koma vilibe cikhulupililo mwa iye . Mofananamo , tingapewe ngozi ngati mwamsanga tadziŵa zilakolako zoipa zimene zingatiloŵetse m’macimo . Komabe , anaganizilanso zimene Yehova anali kuyembekezela kuti iye acite monga kholo . 5 : 8 ; Chiv . Mumalimbitsa ubale mwa kutsatila malangizo akuti : “ Khalani okomelana mtima , acifundo cacikulu , okhululukilana ndi mtima wonse . ” Kodi mukuonapo ciani ? 3 : 6 , 7 . Mulungu anatumiza Mose “ monga wolamulila ndi mpulumutsi kudzela mwa mngelo amene anaonekela kwa iye pacitsamba caminga cija . ” ( Mac . Ngakhale kuti sitinamuonepo kapena kumva mau ake , iye “ amalankhula ” nafe kupitila m’Mau ake ouzilidwa , ndipo ife timafunika kumumvela . ( Yes . Motelo , anthu amene akuloŵa m’banja safunika kukhala na maganizo akuti m’banja mukadzabuka mavuto , adzangothetsa cikwati . — Maliko 10 : 9 . Iye amawalemekeza mwa kuwacha kuti “ ana ” ake . Iwo ali mbali ya banja la Yehova . — Sal . Zimenezo zikanakhala zosiyana na makhalidwe a Mulungu . Peter anakambilana nawo kapepalako na kuwafunsa kuti : “ Kodi moyo wanu mudzaugwilitsa ntchito bwanji ? ” Ndili civalile zovala zanga zakuda zoseŵelela , thukuta lili kamukamu ndinauza Mbonizo kuti , “ Ine Baibulo n’kumanzele . ” Baibo imati : “ Mtima wosangalala ndiwo mankhwala ocilitsa , koma mtima wosweka umaumitsa mafupa . ” — Miyambo 17 : 22 . Ndipo mmodzi wa io anapempha makope 300 a buku lakuti The Harp of God ndi lakuti Deliverance , kuti awaike mu laibulale ya m’ndende . Tingaonetse motani kuti timakonda Mulungu ? 28 : 16 , 30 , 31 . Ndiponso zinthu zikatelo , Mdyelekezi amayamba kutonza Yehova . — Miy . Kodi “ Merozi ” anali ciani ? Mzimayiyo anayamba kunyoza Toñi na kumukalipila poona monga wafika mocedwa kudzasamalila amayi okalamba a mzimayiyo . ( Luka 8 : 3 ) Wolemba mabuku wina anati : “ Luka sananene kuti akaziwo ndiwo anali kuphika zakudya , kucapa zovala , kapena kusoka zovala zong’ambika . Mungaonenso Aroma 10 : 13 ; ndi 1 Timoteyo 1 : 17 . Tisalole cisangalalo ca ka nthawi kutionongela umoyo wathu . N’zoona kuti makanda sangayenelele kubatizika . Yankho ndi lakuti iyai . Yosimbidwa ndi Normand Pelletier Anthu ambili sadziŵa kuti mau opezeka m’ma Baibo ena pa Yohane 7 : 53 – 8 : 11 ni owonjezela cabe , ndipo sali mbali ya Mau a Mulungu ouzilidwa . Atumiki anthawi zonse ambili naonso amamva cimodzimodzi . Ino ndiyo nthawi yophunzila kucitila zinthu pamodzi , cifukwa mgwilizano wotelo udzafunika kwambili mtsogolo . Makambilano amene Yesu anali nao ndi mai wa ku Samariya , amaonetsa mmene Mulungu amaonela kulambila pamalo opatulika kapena mu tuakacisi . Pa sukulu inayake mu Africa muno , gulu la ana a sukulu amene ndi a Mboni za Yehova linakana kucita nao mwambo wolambila mbendela . Nthawi zambili Yesu anagwilitsila nchito mafanizo othandiza anthu kuganiza , owafika pamtima , ndi owathandiza kumakumbukila zimene aphunzila . ( Mat . Komabe , kaya ndife ana , acikulile , olemela , osauka , amphamvu , kapena ofooka , tonse tingathe kuuzako ena zimene timakhulupilila . Mu 1955 , n’napezeka pa misonkhano ya maiko imene inacitikila ku Germany , France , na England . Komabe , sicinali copepuka kuti atumwi aleke tsankho . Paulo anam’patsa udindo wocezela mipingo kuti aithandize ndi kuilimbikitsa , ndiponso kuika abale oyenelela kukhala akulu ndi atumiki othandiza mumpingo . — 1 Timoteyo 5 : 22 . Kale ku Middle East , ubweya wa nkhosa unali kugwilitsidwa nchito kwambili kupangila nsalu mofanana ndi ubweya wa mbuzi ndi ngamila . 30 “ Mukufunika Kupilila ” Mulungu waonetsa kuti amatikonda kwambili mwa kutipatsa Mau ake ouzilidwa . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene Yehova amatithandizila potipatsa ciyembekezo ca mphoto . — Aheb . Ngati zili conco , si zovuta kumvetsa cifukwa cake . Kodi Abulahamu anapindula bwanji cifukwa cokhulupilila Mulungu ? ( b ) Kodi kholo silingathe kucita ciani kwa ana ake ngati limakhala kutali ? M’caka ca 1914 , Yesu Kristu anapatsidwa kolona wakumwamba kutanthauza kuti iye anakhala Mfumu ya Ufumu wa Mulungu . ( Mat . 13 : 19 , 23 ) Ambili amene ndi “ olemedwa ” amatsitsimulidwa mwauzimu pa misonkhano yathu , ndipo mwamsanga amazindikila kuti ‘ zoonadi Mulungu ali pakati pathu . ’ — Mat . Kupuma utsi umenewo kungabweletse matenda a kansa ndi ena . Conco , tiyeni ticite zilizonse zimene tingathe kuti titengele citsanzo cake mwa kucitila ena cifundo . Tikatelo , tidzakhala pa ubwenzi wabwino na Akhristu anzathu komanso ndi anansi athu . — Agal . Kodi kukhala wozindikila kumatanthauza ciani ? Nanga Mkristu wozindikila amalankhula ndi kucita zinthu motani ? M’nkhani iyi , tidzakambilana mafunso amenewa . Malangizo a m’Baibulo amathandiza anthu kukhala ndi makhalidwe abwino . — Ŵelengani 1 Atesalonika 2 : 13 ; 2 Timoteyo 3 : 16 . Ponena za tsogolo lathu , n’ciani cimene Atate wathu wacikondi watiuza ? Ofalitsa ambili ocokela ku maiko ena amene anacitako nchito yapadelayi anaganiza zokukila ku Turkey kuti akathandize pa nchito yaikulu yolalikila imene ili kumeneko . KAMBILANANI NA MNZANU WA M’CIKWATI ( Eks . 33 : 12 - 17 ) Na ise tingalandile madalitso ambili ngati Yehova amatidziŵa bwino . Mkazi wanga anakamba kuti nayenso anali kuganizila za kumene tingakatumikile . ” Zocita zao n’zosiyana kwambili ndi za odzozedwa a Mulungu amene ndi oyela ngati namwali . ( 2 Akor . 11 : 2 ; Yak . 1 : 27 ; Chiv . Conco inuyo ndinu mboni zanga , ndipo ine ndine Mulungu . ” — Yes . Komanso , ngati inu mumakhulupilila zinazake , sizitanthauza kuti nawonso ana anu adzazikhulupilila . Taona kuti nthawi zina mzelawo unali kupitila mwa mwana woyamba kubadwa , koma osati nthawi zonse . Koma ngakhale kuti kuli congo cifukwa ca cimphepo ndi kugwedezeka kwa ngalawa , Yesu akugonabe . Iwo analeke kukoka fodya osati cabe cifukwa codziŵa kuti fodya ndi wovulaza . Baibulo limatiuza kuti pamene Yesu anafuna kusankha amuna 12 kuti akhale otsatila ake , “ anacezela kupemphela kwa Mulungu usiku wonse . ” — Luka 6 : 12 . Tikamaliza , tinali kutumiza zolembazo ku nthambi ya ku Australia kuti akazisindikize . Ena amaganiza kuti akafa adzabwadwanso na kukhala ndi moyo . 3 : 12 , 13 ) Onse anapeleka zifukwa zodzikhululukila , koma zosamveka . Limakambanso kuti anthu adzasangalala ndi moyo wamuyaya . Kodi anthu ena amaganiza ciani ponena za Mulungu ? Ndiyeno , Yesu anacita cozizwitsa . Koma Akristu okhulupilika amene anamvela cenjezo la Yesu anapulumuka . Kodi apa Paulo anali kutanthauza ciani ? Kumbukilani kuti ena mwa abale athu asanaphunzile coonadi , anali na vuto la kumwa kwambili moŵa . Koma lomba ni otsimikiza mtima kupewelatu khalidwe limeneli . Koma palinso zinthu zina zimene Mulungu analosela . ( 2 Akor . 5 : 20 ) Akristu amene ali ndi ciyembekezo codzakhala pano pa dziko lapansi naonso ndi nzika za Ufumu wa Mulungu . Conco , sayenela kutengamo mbali m’mikangano ya m’dzikoli . Tiphunzilanso mfundo zina za m’Baibulo zimene zingatithandize kuthetsa kusamvana kuti tikhalebe paubwenzi wabwino ndi Yehova ndiponso anthu ena . ( 1 Pet . 5 : 10 ) Kudziŵa zimenezi kumatithandiza kuti tisakhale na nkhawa kwambili , ndi kuti tisafooke tikakumana ndi mavuto . Tizikumbukila kuti palibe aliyense amene anali kufunikila cipulumutso . Tonse ndife opanda ungwilo mosasamala kanthu kuti ndife a mtundu wanji . Ngakhale kuti Baibulo silimachula za fodya , ilo limatithandiza kudziŵa mmene Mulungu amaonela kukoka fodya . Pambuyo pake , amuna ake ndi ana awo aamuna aŵili , nawonso anakhala Mboni . Onani zinthu zocepa zimene Yesu , amene anakhala zaka zambilimbili kumwamba ndi Atate ake anafotokoza ponena za Mulungu : Mngelo ameneyu anali kukamba za ‘ amene anapanga kumwamba ndi dziko lapansi . ’ Mbili ya mlongo Lucia Moussanett inalembedwa mu Galamukani ! ( Mat . 24 : 14 ; 28 : 19 , 20 ) Timaonetsanso kuti timakonda kwambili Yehova mwa kukhalabe okhulupilika tikakumana ndi mayeselo . ( Machitidwe 17 : 11 ) Tili ndi zofalitsa zambili zimene zingakuthandizeni kucita zimenezo . Conco , Mulungu nayenso anawakana . Komanso , anakamba kuti anthu adzakhala onenela anzawo zoipa pofuna kuwaipitsila mbili . Tikamasonkhana , timasonyeza kuti tifuna kuyandikila Yehova ndi Mwana wake . ( Luka 17 : 3 , 4 ) Dzifunseni kuti , ‘ Kodi nimaonetsa kuti ndine wokonzeka kukhululukila anthu amene anilakwila , ngakhale amene amanilakwila mobweleza - bweleza ? Dannykarl anati : “ Pafupi - fupi onse pa msonkhanowo anali a m’dziko la Japan , koma ananilandila na manja aŵili , ngati kuti anali kunidziŵa . ” ‘ Kuika Maganizo Athu pa Zinthu za Mzimu Kumabweletsa Moyo na Mtendele , ’ Dec . ( 1 Akorinto 6 : 16 ; Aheberi 13 : 4 ) Kusakhulupilika kumacititsa okwatilana kusadalilana ndipo banja lingayambe kugwedezeka . Pa cifukwa cimeneci , apolisi anali kutifunafuna . Kodi pakhala kusintha kwanji pa kaikidwe ka akulu na atumiki othandiza paudindo ? Ndipo ngati muli na luso linalake , kapena ngati mwacita cina cake cotamandika , muyenela kukumbukila kuti zonse n’zocokela kwa Yehova . Komanso saulula zimene amaseŵenzelapo . Koma zimenezi zimabweletsa mavuto aakulu . Kodi cikondi ndi kupanda tsankho n’zogwilizana bwanji ? Zitanthauzanso kuti muyenela kuyesetsa kukwanilitsa zolinga zauzimu . Mwina mungathandize acinyamata mmene angayambitsile ndi kutsogozela maphunzilo a Baibo . ( Deut . 13 : 12 - 14 ) Akulu amene ali m’komiti ya ciweluzo afunika kupenda mosamala kuti atsimikizile ngati Mkhristu amene anacita chimo lalikulu ni wolapa . Mwina pamene munagwa munadziphweteka dzanja kapena mwendo . Mosiyana ndi anthu ena amene amakhulupilila bodza lakuti adzatamanda Mulungu akadzapita kumwamba , Mboni za Yehova panthawi ino zikutamanda Mulungu pano padziko lapansi . Onani mmene Akristu akale anacitila pamene mumpingo wao munabuka mikangano . Konzekelani . Panena kuti : “ Ndiponso aliyense amene afuna kukwatila ayenela kukhala wokonzeka kusamalila zofuna za mnzakeyo . Yesu ndiye Mtsogoleli wathu , ndipo tiyenela kutsatila iye yekha cabe Pambuyo pokamba za kuikiwa m’manda kwa Yesu , Baibo siikambakonso za Yosefe wa ku Arimateya . Kumeneko iye anawafotokozela mwatsatanetsatane mmene Saulo anaonela Ambuye . . . pamseu . Anawafotokozelanso mmene Saulo analankhulila molimba mtima ku Damasiko m’dzina la Yesu . ” ( Mac . 11 : 3 ) Koma amuna ndi akazi ena akaloŵa m’banja , zimawavuta kutsatila dongosolo limeneli . Abale anasonkhana m’ndende yonzunzilako anthu ku Mordvinia , m’dziko la Russia kuti acite mwambo wa Cikumbutso mu 1957 “ Kugwilizana n’kofunika kwambili m’cikwati . Tiziona mipata yolimbikitsila ena . N’ciani cingatithandize kukhala otsimikiza mtima kuti cikondi ca Yehova kwa ife n’cosatha ? Komabe , iwo anali ofunitsitsa kulalikila uthenga wabwino . 3 : 16 , 17 . Kodi Mulungu angakuthandizeni pa mavuto anu mukam’pempha mogwilizana ndi cifunilo cake ? Kucokela mu 1500 B.C.E . , pamene malemba opatulika anayamba kulembedwa , thandizo lakhala likupelekedwa n’colinga cakuti anthu amvetsetse malemba . Abale acikulile , pewani nsanje yakaduka . Munthu wodzicepetsa amalemekeza Yehova , cifukwa ni Mlengi wathu , komanso ni Mfumu ya Cilengwedwe Conse . Ngakhale kuti Malemba safotokoza mwatsatanetsatane mmene anali kuikila abale pa udindo , tingathe kuona mmene zimenezi zinali kucitikila . Koma pali anthu ena amene aonetsa kuti ali na cikhulupililo colimba mwa Mulungu . Mulungu sanapange munthu woyamba kucokela ku nyama koma ku fumbi lapansi . — Ŵelengani Genesis 1 : 24 ; 2 : 7 . Kodi Yesu anapeleka citsanzo cabwino citi ca kudzimana ? Ndipo caka na caka , banja lokhulupilika limeneli lakhala likulalikila uthenga wa Ufumu pamalowa m’maŵa uliwonse , kwa masiku 6 pa wiki . 6 : 6 , 7 . Ngati takamba zinthu panthawi yolakwika , anthu sangamvetsetse zimene takamba kapena kuzivomeleza . 61 : 8 . Ndi zinthu ziti zimene zingatikhumudwitse ? Nanga n’ciani cingatithandize kuti tiziona utumiki wathu moyenelela ? Conco anaganiza zopanga cosankha cakuti azikoka fodya pamaso pa mmishonale uja kapena kusiilatu kukoka . Nanga nidzathana nayo bwanji nikadzakwatila ? ” M’bale Stephen asanayankhe funso limenelo , anapempha Eduardo kuti aganizilenso mau ena amene mtumwi Paulo analemba akuti , Yehova ni “ Mulungu amene amatitonthoza m’njila iliyonse , amenenso amatitonthoza m’masautso athu onse . ” — 2 Akor . Motelo , n’zoonekelatu kuti Yesu , Mwana wa munthu , anali “ wodzicepetsa . ” — Mat . Mukaima , nayenso aima . Komanso mkulu wanga , mkazi wake ndi ana ake tsopano ndi Mboni za Yehova . Ndiponso , sicinali copepuka kuleka makhalidwe oipa . Onani kuti Yehova sanamudzudzule Eliya , koma anam’thandiza . Monga mmene Yesu analonjezela , tsiku lidzafika pamene onse amene Mulungu akuwakumbukila adzamva mau a Khiristu , ndipo adzauka ndi kukhala m’dziko lokongola ndi lamtendele . — Yohane 5 : 28 , 29 . Ndithudi , kupeleka moni modzicepetsa kungathandize munthu kukhala womasuka musanayambe kukamba naye nkhani yaikulu . Kodi makadi a ulaliki anali othandiza bwanji ? Ndipo Mulungu anali kudzam’thandiza kuti apeleke uthenga wake kwa Farao . Ndi citsanzo citi cimene cionetsa kuti Yesu anali kukamba m’njila yosavuta kumva ? ( Chivumbulutso 12 : 9 , 12 ) Kuonjezela pamenepa , tikutsatila lamulo la Yesu mwa kulalikila anthu ambili padziko lonse lapansi m’zinenelo zambili kuposa kale lonse ! Abale ambili ali ndi maganizo ofanana ndi a mabanja aŵili a ku Florida omwe ali ndi zaka za m’ma 50 . Oipa akadzacotsedwa , n’ndani adzakhala padziko ? 14 : 8 . Kuwonjezela apo , anthu ambili amaona kuti ziphuphu zaculuka ngako padziko . ( Salimo 139 : 4 ) Conco , n’cifukwa ciani tiyenela kupemphela kwa Mulungu ? ( Maliko 1 : 38 ; 13 : 10 ) Yesu anagwilitsila nchito Mau a Mulungu pophunzitsa . Kodi Akhristu ofikapo amalimbikitsa bwanji mgwilizano mumpingo ? ( Yakobo 3 : 5 ) N’cifukwa ciani Yakobo anakamba mau amenewa ? Mmodzi wa abale amenewa ndi Bill wa ku Australia . Kodi zinthu zinamuyendela bwanji ? “ Pelekani zinthu . . . za Mulungu , kwa Mulungu . ” — MATEYU 22 : 21 . 26 : 19 ; Hos . ( Aroma 12 : 18 ) Citani zonse zimene mungathe kuti mulimbikitse mtendele na mgwilizano . Kudalilana kumeneko ndi kocititsa cidwi kwambili . Inoki ni wakufa mpaka lelo , koma Yehova , Mulungu amene amakwanitsa kukumbukila ciliconse , akali kumukumbukilabe . Muzitsatila malangizo atsopano mosamala . Koma pemphelo langa silinayankhidwe . ” — Samuel , * wa ku Kenya . Arthur Willis ndi Bill Newlands anali aŵili mwa apainiya akhama ofunitsitsa kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu kumadela ambili akutali m’dziko la Australia . M’Baibulo , kupilila kumatanthauza zambili osati cabe kulolela kuvutika . Muzikhululukila ena na mtima wonse . Masiku ano , zimene timatsatila pankhani ya cikwati , zingakhale zosiyanako . [ 2 ] ( ndime 9 ) M’buku la Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu masamba 62 - 64 , muli malangizo othandiza a mmene mungayambile kukambilana na anthu . Komabe , Baibulo limatitsimikizila kuti : “ Mulungu si wosalungama woti angaiŵale nchito yanu ndi cikondi cimene munacisonyeza pa dzina lake , mwa kutumikila oyela ndipo mukupitiliza kuwatumikila . ” ( Aheb . Sikuti utsogoleli wa Yesu unali wa zaka zocepa cabe . Nthawi zina , mtendele pakati pa abale umataika cifukwa bizinesi imene anapangana siinayende bwino kupangitsa wina kuluza ndalama zake , mwinanso cifukwa wina wadyela mnzake masuku pamutu . 37 : 15 - 17 . Kodi ndidzakhala m’ndende muno mpaka liti ? ’ Njila yabwino kwambili yocitila zimenezi ni kuwaphunzitsa za Mulungu ndi zimene Ufumu wake udzacitila anthu . Koma makolo athu sanaleme nafe . ” Tingaphunzile zambili kwa Yesu cifukwa iye anati : “ Ine ndine wocokela kumwamba . ” — Yohane 8 : 23 . Kodi nimayesa kupewa “ nchito za thupi , ” monga mkwiyo ndi mkangano ? — Agal . Atumiki a Mulungu a masiku ano naonso akuyembekezela kukwanilitsidwa kwa maulosi ena okhudza Mesiya . Yesu anali kusankha mabwenzi ake mosamala kwambili . Ngati tifunitsitsa kwambili cinthu cina cake , monga ndalama zambili kapena zinthu zina zapamwamba , zinthuzo zingayambe kulamulila moyo wathu ndi kukhala mulungu wathu . Timoteyo anali kucita zinthu mogwilizana ndi tanthauzo la dzina lake limene limatanthauza kuti , “ Munthu Amene Amalemekeza Mulungu . ” Pelekani citsanzo ca m’Baibulo . Nkhaniyo inandilimbikitsa kupitiliza utumiki wanga . ” — Salimo 44 : 25 , 26 ; Yesaya 41 : 10 , 13 . ( 2 Tim . 3 : 1 - 4 ) Vuto lina ndi lakuti mdani wankhanza ndi wofunitsitsa kuononga mabanja . Ngati Yesu sanafe ndi kuuka , sitikanamasulidwa ku cilango ca ucimo ndi imfa . Kucita zimenezo kunali kunicititsa kukhala na cidalilo na kudziona kuti ningathe kucita zinthu ngati anthu ena onse . Angelines ndi mwamuna wake anandipempha mobwelezabweleza kuti ndiziphunzila nao Baibulo . Koma mfundo za m’Baibo zingatithandize kupewa mavuto amenewo mwa kudziŵa zimene zimaayambitsa , monga kuceza kokopana na kutamba zamalisece . Kuthandiza Ana a Alendo Ocokela m’Dziko Lina , May Zimene anakuphunzitsani zakuthandizani kukhala ndi nzelu ‘ kuti mudzapulumuke kudzela m’cikhulupililo cokhudza Kristu Yesu . ’ 1 : 13 , 14 ; Akol . Kuonjezela apo , anthu amene timakumana nao mu ulaliki naonso ndi anzathu . ( Yoh . 12 : 31 ; 14 : 30 ; 16 : 11 ) Yesu anali kudziŵa kuti Mdyelekezi adzacititsa anthu kukhala mum’dima wa kuuzimu n’colinga cakuti asaone kuti maulosi amene Mulungu anakamba ali pafupi kukwanilitsika . ( Zef . Naphunzila zambili mu utumiki umenewu . Koma cacikulu n’cakuti nadzionela nekha kuti Yesu Khristu , osati munthu , ndiyedi mutu wa mpingo wacikhristu . Kodi tifunika kucita ciani kuti Mulungu azitithandiza ? Pali abale na alongo ambili amene angakutsimikizileni kuti pemphelo limawathandiza . yomwe ili m’magazini ino . Chechi ndiye inali kugamula cilango ca kunyongewa , Boma ndiye inali kunyonga anthu . Dziko linafuna kuticotsa kwa Yehova , koma titaona kuti makolo athu akuika patsogolo zinthu za kuuzimu , nafenso tinayesa kucita cimodzimodzi . Maboma ena amakonza pulogilamu yothandiza anthu othaŵa kwawo kuti ajaile umoyo watsopano . 14 Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga Yesu anapeleka fanizo limene lionetsa kuti Afarisi sanali kucitila cifundo anthu olakwa . Anthu akayamba kuphunzila Baibo , ambili amaŵelenga nkhani za anthu akale amene anaukitsidwa , monga za kuukitsidwa kwa Lazaro . ( Yohane 8 : 44 ) Kukhulupilika kwawo kwa Mulungu kumatikumbutsa Aisraeli olapa amene anati : “ Inu Yehova , inu ndinu Atate wathu . Kuwonjezela pa kulalikila , kodi tingaonetse kuwala kwathu m’njila zina ziti ? Zimenezi zinatiphunzitsa kuti tikafika kudela latsopano , ndi bwino kuti tisamalalikile m’delalo . M’nthawi ya oweluza aciisiraeli , mneneli wamkazi Debora anathandizidwa ndi Mulungu . Iwo anakondwela ngako na zimene anaŵelenga m’mabukuwo . Mofanana ndi abale ena amene anali m’gulu lovomelezedwa ndi likulu , naonso anaikidwa m’ndende cifukwa cosatenga mbali m’zandale . Koma Inoki , ngakhale kuti anali wopanda ungwilo , anayenda ndi Mulungu ndipo anasiyila mbadwa zake citsanzo cabwino ca cikhulupililo . Satana ndiye “ wolamulila wa dzikoli ” ndipo lili m’manja mwake . ( Yoh . Zinthu zimenezi ndi ( 1 ) cilengedwe cake , ( 2 ) Mau ake ouzilidwa , ( 3 ) pemphelo , ndi ( 4 ) dipo . Ngati okwatilana ndi okhulupilika ndipo amagonjela Yehova , cikwati cao cidzakhala ndi maziko olimba . Komabe , mogwilizana ndi kukwanilitsidwa kwa ulosi umenewu , pamapeto pa masiku atatu ndi hafu , mboni ziŵili zimenezo zinaukitsidwa . Anthu oposa wani miliyoni anali atafa pankhondo m’dziko la France . Conco kunali kufunikila anthu ambili ogwila nchito m’migodi ya malasha . Ndipo monga mmene zinalili ndi Elisa , inu ophunzila okhulupilika , Yehova angakuthandizeni kucita zinthu zazikulu kuposa aphunzitsi anu . — Yoh . 14 : 12 . Panthawiyo , mneneli Eliya anawauza momveka bwino kuti asankhepo pakati pa kutumikila Yehova kapena kutumikila Baala , mulungu wonama . ( 1 Maf . Conco mu 2004 , iye anayankha funso lofunika kwambili limene sanafunsidwepo lakuti , kodi wadzipeleka kwa Mulungu kucita cifunilo cake ? “ Onse amene anali kumumvetsela anadabwa kwambili ndi mayankho ake komanso poona kuti anali womvetsa zinthu kwambili . ” Rodney na mkazi wake Jane , amene anacokela ku Australia , ndipo ni a zaka za m’ma 50 , akhala akutumikila ku Myanmar kuyambila mu 2010 pamodzi ndi ana awo Jordan na Danica . Izi zinacititsa kuti niphunzilenso zinthu zina zambili . Ndipo Akristu onse ayenela kutsatila malangizo amenewa . 13 Mbili Yanga ​ — Nakhala na Mwayi Wotumikila Pamodzi ndi Amuna Auzimu Kodi Yehova Waonetsa Bwanji Kuti Amatikonda ? Kunyada nthawi zina kumacititsa anthu kusankhana mitundu . Yelekezaninso kuti mukukhala m’dziko lopanda zipatala , madokota , manesi , makampani a inshuwalansi ya za umoyo , mamochale , nyumba za malilo , amalukula , kapena manda . Akadzamupempha madzi akumwa , iye adzapatse Eliezere madzi ndi kumwetsa ngamila zake zonse . Mu 1587 , Hutter anatulutsa Baibo ya Ciheberi imene imadziŵika kwambili kuti Cipangano Cakale . Kodi ticite kukutulutsilani madzi m’thanthweli ? ” N’cifukwa ciani zinali zovuta kuti ophunzila a Yesu alalikile uthenga wabwino “ ku mitundu yonse ” ? M’malomwake , muyenela kutsatila Mau a Mulungu amene amati : “ Wocenjela ndi amene amati akaona tsoka amabisala , koma anthu osadziŵa zinthu amangopitabe ndipo amalangidwa . ” — Miy . Kumbukilani kuti mau a Yesu apa Yohane 3 : 16 , amafotokoza bwino kuti “ wokhulupilila ” mwa iye adzapulumutsidwa . TENGELANI CIKHULUPILILO CAWO SARA Pokonzekela , mungayambe mwa kufufuza yankho ya funso imene anzanu amakonda kufunsa ku sukulu . Ŵelengani na kusinkha - sinkha Malemba okamba za kufunika kwa Cikumbutso . Jeffery amene anali kucita zamalonda , anati : “ Nditapita patsogolo kuphunzila Baibulo , ndinazindikila kuti sindiyenela kucita cinyengo pocita pangano la zamalonda . Inde , tifunika kukumbukila kuti anthu amasiyana - siyana , ndipo tiyenela kusintha - sintha ulaliki wathu kuti ugwilizane na munthu amene tikamba naye . — 1 Akor . TSAMBA 7 • NYIMBO : 28 , 107 Cifukwa cakuti colinga ca aja amene afuna kutumikila monga akulu ndico kucita “ nchito yabwino ” osati kupeza mpando . Lemba la Miyambo 1 : 5 , limati : “ Munthu wanzelu amamvetsela ndi kuphunzila malangizo owonjezeleka . ” ( 2 ) Yehova ndi mtetezi wathu , ndipo ( 3 ) Mulungu ndi bwenzi lathu lapamtima . Kodi tiyenela kukumbukila ciani tikapeza munthu waukali mu ulaliki ? ( Sal . 119 : 9 ) Mau a Mulungu ali ndi malangizo ofunika amene angatithandize kusiyanitsa nkhani zoona ndi zabodza . Nthawi zonse muzikumbukila kuti Yehova amatilangiza cifukwa amatikonda . — Salimo 30 : 5 . ( Mlaliki 9 : 11 ) Komabe , kuti mukakhale na moyo wamuyaya , zimadalila pa zosankha zanu maka - maka . Mwa nzelu zake , Yehova sanatiuze dzina leni - leni la mngelo amene anam’pandukila . Kodi Yakobo akanakwanitsadi kulimbana ndi mngelo wamphamvuyo ? ( a ) Kodi kapolo wokhulupilika waonetsa bwanji kuti ali maso kwambili pofotokoza nkhani zina za m’Baibulo ? ( 1 Mbiri 29 : 11 ; Mac . 4 : 24 ) Pa Chivumbulutso 4 : 11 , a 144,000 amene adzalamulila pamodzi na Khristu kumwamba anaonekela m’masomphenya akukamba kuti : “ Ndinu woyenela , inu Yehova Mulungu wathu wamphamvu , kulandila ulemelelo ndi ulemu , cifukwa munalenga zinthu zonse , ndipo mwa kufuna kwanu , zinakhalapo ndipo zinalengedwa . ” Pambuyo pa Ulamulilo wa Kristu wa Zaka 1,000 , cifunilo ca Yehova cokhudza dziko lapansi cidzakwanilitsidwa . Ndipo pamapeto pake iwo sadzakhalanso na mphamvu pa zandale ndi pa za cipembedzo . Iwo anasautsa moyo wa Aisiraeliwo powagwilitsa nchito yoŵaŵa yaukapolo , yomwe inali yoponda matope ndi kuumba njerwa . Komabe , sitiyenela kuganiza kuti iye amalekelela makhalidwe oipa . Koma ngati tisonkhela nkhuni kaŵilikaŵili motowo umapitiliza kuyaka . Ndiyeno , mau a m’fanizo la Yesu akuti : “ Sangalala limodzi ndi ine mbuye wako , ” angagwilenso nchito kwa inu . — Mat . A Yohane : Ohoo ! Conco , ndi kwanzelu kusatengela tsankho limene lafala m’dzikoli . Nthawi zambili , n’nali kukhala wolusa cakuti anzanga ena anali kuniopa cifukwa ca khalidwe laciwawa . Kuwonjezela apo , olemba Malemba Acigiliki Acikhristu anachula za Abulahamu nthawi zoposa 70 . Anthu ambili amatenga mbali m’zandale cifukwa coona zinthu zopanda cilungamo zimene zicitika . Gulaye anali cida cothandiza kwambili moti nthawi zina panali kukhala gulu la asilikali ogwilitsila nchito gulaye . 5 : 23 ) Molingana ndi bungwe lomulila la m’nthawi ya atumwi , kapolo ameneyu amatsatila mau ouzilidwa a Mulungu , ndipo amawalemekeza ngako . Tidziŵa kuti mulimonse mmene zinthu zingakhalile , Yehova sadzalephela kukwanilitsa colinga cake , ndipo nthawi zina amacita zinthu m’njila imene sitinali kuyembekezela . Mabaibulo amene anali atamasulidwa kale m’zinenelo zina , anathandizanso pa nchito yokonzanso Baibulo latsopano la Cingelezi . — Miyambo 27 : 17 . A Zimba : Inde ukugwilizana . Cifukwa cakuti cikondi ndi khalidwe lalikulu la Yehova , ndipo anatilenga m’njila yakuti tizitha kutengela cikondi cake . ( Gen . Ine ndi mkazi wanga tapeza cimwemwe ceni - ceni cifukwa cogwila nchitoyi . ( b ) Kodi kukonda abale athu kumagwilizana bwanji ndi kukonda Mulungu na Baibo ? ( Luka 4 : 22 ) Pamene munthu wina wa cuma anafuna kulemekeza Yesu mwa kukamba kuti , “ Mphunzitsi Wabwino , ” modzicepetsa Yesu anamuyankha kuti : “ N’cifukwa ciani ukundichula kuti wabwino ? Nanga cifukwa ciani ? Makolo Acikhiristu amacita bwino kuonetsetsa kuti Mau a Mulungu akufika pamtima pa ana awo . Kufunsa funso limeneli kungamuthandize kudziŵa zimene angacite kuti atumikile Mulungu ndi mtima wonse . ( 1 Pet . 5 : 2 ) M’caka ca 1976 , Bungwe Lolamulila linalinganizidwa kukhala makomiti 6 n’colinga cakuti aziyang’anila nchito ya Ufumu padziko lonse lapansi . Pamisonkhano yacigawo , m’matenti a kafiteliya anali kuikamo mathebulo akuluakulu aatali . Anthu anali kuimilila pamenepo ndi kudya msangamsanga kuti asiyile ena malo . Zakalezo zapita . ” Komabe , Mulungu , amene dzina lake ndi Yehova , safuna cabe kuti timasuke ku zizoloŵezi zoipa zimene zimaononga thupi lathu . N’kutheka kuti inali nthawi imeneyi pamene iye anapeleka lamulo lakuti : “ Conco pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse kuti akhale ophunzila anga . Muziwabatiza m’dzina la Atate , ndi la Mwana , ndi la mzimu woyela , ndi kuwaphunzitsa kusunga zinthu zonse zimene ndinakulamulilani . ” ( Mat . 28 : 19 , 20 ; 1 Akor . Mwacitsanzo , kudzela m’Baibulo , Mulungu watiuza mmene tiyenela kuonela magazi , ndipo timamvela zimenezo . Baraki anafunika kusonkhanitsa amuna 10,000 kucokela m’mafuko aŵili a Isiraeli . Poganizila zocita , iye anati : “ Ndinapemphela kwa Yehova mosalekeza kuti andithandize kusankha zinthu mwanzelu . ” Ndife gulu lapadziko lonse ndipo sitigwilizana ndi magulu aliwonse a zipembedzo . M’nthawi za Yesu , anthu ambili anali osauka . Mwina io anaganiza kuti kukhala ndi ndalama kukanacititsa kuti akhale ndi umoyo wabwino ndi wotetezeka . Ngati munthu wataikilidwa uzimu wake , amapeleka mpata wakuti “ mpweya ” woipa kapena kuti mzimu wa dzikoli uloŵe mwa iye . Nikanakonda kukhalabe mu utumiki umenewo . Umu ni mmene uphungu wamphamvu ndi wolimbikitsa wa Yehova unam’khudzila Yobu . 1 : 6 , 16 ) Koma Luka aoneka kuti anachula maina a makolo a Mariya ndi kuonetsa kuti Yesu anali na ufulu wobadwa nawo woloŵa ufumu wa Davide . Anali kuyankha mafunso amene ndinali kuwafunsa . ( Maliko 12 : 30 ) Aliyense amene afuna kubatizidwa ayenela kukhala wokonzeka kusunga lonjezo lake kwa Yehova . — Ŵelengani Mlaliki 5 : 4 , 5 . Madokotala ena amaonanso kuti pemphelo ndi “ njila ina yocilitsila . ” 4 Mphatso ya Mulungu Yopambana Zonse — N’cifukwa Ciani ni Yamtengo Wapatali ? N’ciani cimene Yehova amafuna kuti makolo azicita ? Iwo amayamikila kuti Mboni za Yehova zimawafikila panyumba zao . Ndidzamuteteza cifukwa wadziwa dzina langa . ” Zoona n’zakuti nthawi imeneyo , Cikhiristu campatuko cinagwilizana na zipembedzo zacikunja za mu Ufumu wa Roma . Zipembedzo zonsezo zinapanga Babulo Wamkulu . Komabe , panali Akhiristu odzozedwa ocepa amene anali monga tiligu . Mu 1945 , kunacitika ngozi yoopsa pa madzi pamene ngalawa yochedwa Wilhelm Gustloff inamila ndipo anthu masauzande ambili anafa . 40 : 8 ; 119 : 97 ) Kuwonjezela apo , tiyenela kuyesetsa kupewa zinthu zimene zingatilepheletse kukhala anthu auzimu . — Tito 2 : 11 , 12 . NYIMBO : 60 , 38 Mwina mungazengeleze kudziyesa , maka - maka ngati muona kuti mudzalephela kucita zimenezo . ( Miy . 31 : 10 - 31 ) Kugonjela mwacikondi kumeneku kumacititsa kuti m’banja mukhale cimwemwe , mtendele , ndi mgwilizano . Pambuyo pa zaka ziŵili , m’caka ca 2007 , ndinapita ku Mongolia . Koma m’zaka zaposacedwapa mabuku athu safotokoza kwambili zimenezo . Baibulo limatiuza kuti umphawi wavutitsa anthu kwa nthawi yaitali . — Ŵelengani Yohane 12 : 8 . Elizabeth Fot ; Aksamai Sultanalieva Kodi zimene anthu ena amakamba zakuti kulibe Mlengi n’zoona ? Ngakhale n’conco , izi sizitilepheletsa kutamanda Atate wathu Yehova mogwilizana . ( 2 Maf . 2 : 15 ) Mkati mwa utumiki wake wa zaka 60 monga mneneli , Yehova anathandiza Elisa kucita zozizwitsa zambili kuposa zimene Eliya anacita . Amadziŵa zofooka zathu , zimene tingakwanitse kucita , ndi mmene tapitila patsogolo , ndipo amaganizila zimenezi akamatiumba . Ndife odala kwambili cifukwa Yehova watipatsa nchito imene imatibweletsela cimwemwe , imatithandiza kuti tikhale pa ubwenzi wolimba ndi Mulungu ndiponso abale athu , komanso imateteza ubwenzi wathu ndi iye . • Kodi zoipa zimangocitika mwangozi , kapena munthu ndiye amazicititsa ? Mulungu amathandiza ndi kudalitsa onse amene amam’tumikila ndi zolinga zabwino . Fotokozani zitsanzo zoonetsa tsankho limene anthu anaonetsa kwa Yesu . Anthu a Yehova ndi ogwilizana kwambili masiku otsiliza ano kuposa kale . Ngakhale n’conco , mungathe kukhala ndi umoyo wacimwemwe ndi kumatumikila Yehova mosangalala . Iye anati : “ Cimene cinandithandiza kwambili ndi kufuna kukondweletsa Yehova . ( Luka 21 : 20 ) Koma mwina io anali kudzifunsa kuti , ‘ Tidzatsatila bwanji cenjezo la Yesu limeneli ? ’ Pamenepa tinazindikila kuti tinalidi kukhomeleza mfundo za coonadi m’mitima ya ana athu . Kodi Madison amacita ciani kuti asagonje ? Tiyeni ticite zimene tingathe kuti tithandize anthu kuti akapulumuke pamene dzikoli likuonongedwa . Fotokozani makonzedwe apadela okhudza kuimba amene Nehemiya anakonza pamene anali bwanamkubwa ku Yerusalemu . Kodi ophunzila masiku ano mukutengapo phunzilo lotani ? ( a ) Kodi Yehova anapeleka malangizo otani kwa Aisiraeli m’mwezi wa Nisani mu 1513 B.C.E . ? Kuonjezela pamenepo , anzake atatu a Danieli anakana kugwadila fano la golide limene Nebukadinezara anapanga . Palinso zinthu zina zimene tingacite kuti tipilile . Amacita zimenezi mwa kulalikila uthenga wabwino ndi kuphunzitsa a “ nkhosa zina ” mamiliyoni ambili njila za Yehova . ( Yoh . Ndi nkhani iti imene Akristu ayenela kutengako mbali ? Kodi kuvala umunthu watsopano kumalimbitsa bwanji cikwati ? Wokwelapo akuimila nkhondo . ( b ) N’cifukwa ciani ubatizo ukuyelekezeledwa na nchito yomanga cingalawa imene Nowa anacita ? N’nali kudziona wacabe - cabe cifukwa colemala komanso cifukwa cokulila m’nyumba ya olemala . Yehova Mulungu , amene anapanga Paradaiso woyambilila , analonjeza kuti adzabwelezeletsa zimene zinataika . Koma malinga n’zimene takambilana , pali umboni wokwanila wakuti iye anayamba kudzidziŵikitsa kuti ni Mkhristu . Ndi malangizo ena ati a m’Baibulo amene angatithandize kusankha mwanzelu pankhani ya cithandizo ca mankhwala ? Kodi sanaone kuopsa kwa zimene anacita ? “ Adzakhala ansembe a Mulungu ndi a Khiristu , ndipo adzalamulila monga mafumu limodzi naye . ” — Chivumbulutso 20 : 6 . Cikondi ca Akhiristu ali pabanja ciyenela kukhala camphamvu , moti aliyense afunika kukhala wokonzeka kufela mnzake . Ndipo musaiŵale kuti Yesu anatiphunzitsa kuti tikayandikila Atate wathu Yehova , tidzakhala osangalala kwambili . Conco , kumvetsetsa buku la Levitiko kudzatithandiza kupewa kucita ciliconse cimene cingabweletse citonzo pa dzina la Mulungu . ( 1 Akor . 11 : 2 ) Koma akaona kuti pena pake sanacite bwino , anali kuwauza mokoma mtima ndi momveka bwino cifukwa cake anafunika kuwongolela . — 1 Akor . Cacitatu , m’bale amene akalamila udindo afunika kuonetsa makhalidwe amene mzimu woyela wa Mulungu umatulutsa . ( Agal . Kodi Cilamulo ca Mulungu kwa Aisiraeli Cinali Colungama ndi Cosakondela ? Ofalitsa ena okalamba amalalikila atakhala m’mbali mwa mseu kapena pa sitesheni ya basi . Iye anacita zimene anakwanitsa ndipo zimenezi zikutiphunzitsa cinacake . Tikamacita zimenezi , tidzapulumuka cisautso cacikulu ndi kusangalala cifukwa cophunzila za Yehova Mulungu wathu wanzelu ndi wacikondi kwamuyaya . — Mlaliki 3 : 11 ; Aroma 11 : 33 . Timafuna kuonetsa cikondi kwa anzathu m’njila yapadela . Kodi aliyense wa ife angakondweletse bwanji Yehova ? Kodi pangakhale zotulukapo zabwanji ngati mwamunayo wadziŵa kuti mkazi wake anali kumubisa zinazake ? Ngati yankho lanu ndi iyai , ndiye kuti mwayankha bwino . 1 , 2 . ( a ) Kodi anthu ali na maganizo osiyana - siyana ati pa nkhani ya ufulu wosankha zocita ? Mfundo zina pankhani yoloŵa nchito imene imafuna kunyamula mfuti kapena zida zina , mungazipeze mu Nsanja ya Olonda ya November 1 , 2005 , peji 31 , ndi Nsanja ya Cizungu ya July 15 , 1983 , mapeji 25 - 26 . . Podzafika m’nthawi imene Alexander Wamkulu anagonjetsa cigawo ca Middle East mu 332 B.C.E . , akatswili acigiriki anali atafalitsa ciphunzitso cimeneci , ndipo m’kupita kwa nthawi cinafalikila mu Ufumu wa Girisi . Sitidzafunikila kucita mantha . ( a ) Kodi mabuku athu ofotokoza Baibulo asintha bwanji kuyambila mu 1919 ? Anali woipa m’maonekedwe , ndipo anali kukonda kuopseza anthu . Izi zingafanane ndi mmene tingaonetsele munthu madela ena a dziko lapansi pogwilitsila nchito TV . Cifukwa cakuti sanalamulile mkwiyo wake , iye anapha m’bale wake wokhulupilika Abele . Ni zinthu ziti zimene Asa anacita molimba mtima ? Iye amatengelapo mwayi pa zimene wofunsilayo wamuululila mosadziwa , ndiyeno woloselayo amadziŵa zeni - zeni zokhudza munthuyo na mmene zinthu zilili mu umoyo wake . Iye anasintha mothandizidwa ndi Yehova ndiponso mphamvu ya Mau a Mulungu , Baibulo . — Aheberi 4 : 12 . Patapita nthawi , tinapita kukasonkhana ku mpingo wina umene sunali monga kilabu ya nkhalamba , koma unali na acicepele ambili . NKHANI YA PACIKUTO | KODI TINGAPEZE KUTI CITONTHOZO ? Koma tiyenela kuona zinthu mmene Mulungu amazionela . ( Mika 7 : 7 ) Yehova amathandiza atumiki ake okhulupilika ngakhale kuti nthawi zina amawalola kuyembekezela kuti apatsidwe udindo wina wake , kapena kuti zinthu zisinthe . Anthu ambili masiku ano akukhamukila kwa Yehova kuti am’lambile pamodzi ndi anthu ake . Izi zinanenedwelatu ndi aneneli aŵili akale . Fotokozelani wophunzila cifukwa ca m’Malemba pa zimene mwamupempha kucita . Kupandukila Yehova kumatsogolela ku imfa , ndipo tizikumbukilanso kuti “ kunyada kumafikitsa munthu ku cionongeko . ” — Miy . 7 : 9 , 10 . 5 : 29 ) Koma iye afunikanso kuganizila mfundo yakuti mkazi afunika kukhala wogonjela ndi wololela . ( Aef . Patapita zaka zambili , mfumu ya ku Iguputo inaika Yosefe kukhala munthu waciŵili wapamwamba kwambili m’dzikolo cifukwa cakuti inacita cidwi ndi luso lake pa nchito . Baibulo sililetsa anthu kugwila nchito mwamphamvu . N’zacisoni kuti angelo ena anasankha kupandukila Mulungu . — Yuda 6 . Anali kutitenga kuti tikadye nawo cakudya camadzulo , koma anali kucita izi kukafipa . ( Num . 20 : 6 - 8 ) Koma Mose sanakambe nalo thanthwelo . Mtendele wa Aroma , mayendedwe osavuta , cinenelo cofala , lamulo la Aroma , ndiponso Ayuda okhala m’maiko ena , zinathandiza ophunzila a Yesu kupitiliza kugwila nchito yolalikila imene Mulungu anawapatsa . Kuyambila nthawiyi , n’nakhala na colinga cophunzila zambili zokhudza Baibo . Conco , n’navomela kuti aziniphunzitsa Baibo . MBILI YANGA Magulu ankhondo a angelo kumwamba adzathandiza Yesu Khristu , Mfumu ya Mafumu , kumenya ‘ nkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu Wamphamvuyonse ’ pa Aramagedo . Nanga mungawathandizenso bwanji kukhala na cikhulupililo colimba ? Komabe , Sara anali wokonzeka kusiya malo amene anajaila . Mulungu anauza Adamu kuti : “ Tsiku limene udzadya , [ za mtengo wodziŵitsa cabwino ndi coipa ] udzafa ndithu . ” Nkhani iyi ya m’Baibo imatiuza kuti banja la Abulahamu linasamuka ndi cuma cimene anapeza ndiponso “ akapolo awo onse amene anapeza kudziko la Harana . ” Kukambilana nawo pa nthawi ngati imeneyi , kwatithandiza kuti tizikambilana momasuka . ” — Nicole . 31 : 15 ) , 12 / 15 ( Yoh . 4 : 9 , 27 ) Pa nthawiyo , atsogoleli acipembedzo aciyuda sanali kukamba na akazi pa gulu . Yehova anaveka Mwana wake , Yesu Kristu , cisoti cacifumu monga Mfumu Mesiya mu 1914 . “ Ine Ndili Ndi Ciyembekezo mwa Mulungu , ” Dec . Tinali kukhala na umoyo wosaukila cifukwa nthawi imeneyo kunali mavuto aakulu a zacuma . Kwa kanthawi , n’natumikilako mu Dipatimenti ya Utumiki ndiponso monga mlangizi wa masukulu osiyana - siyana . ( 1 Mafumu 20 ) Panthawiyo Ahabu ndi Yezebeli anakhala adyela , okonda cuma ndi ankhanza kwambili kuposa ndi kale lonse . Inenso n’nagwetsa misozi yacimwemwe . Posapita nthawi , Tyndale ananyongedwa ndi kutenthedwa pamtengo . Tingaphunzile zambili pa nkhaniyi mwa kuona mmene Yesu anacitila zinthu m’nthawi yake pamene kunali mavuto a zandale . 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani dzikoli lili ngati cigaŵenga cimene cipita kukanyongedwa ? A Mboni za Yehova ni okonzeka kukuthandizani kuphunzila Baibo . Kodi muli naye mnzanu wotelo ? Amapewa kutenga mbali m’ndale ngakhale kuti kucita zimenezo kungacititse kuti akhale ndi ndalama zocepa kapena asakhale ndi ciliconse . — Aheberi 10 : 34 . Pa nkhani imeneyi , pulofesa John A . Inoki analengeza uthenga wa Mulungu molimba mtima kwa anthu aciwawa Yehova amakonda anthu amene amacititsa kuti iye atamandike mwa kutengela makhalidwe ake apamwamba , kuphatikizapo khalidwe la kukhala oona mtima . Mau a pa Miyambo 3 : 5 , 6 , ni oona amene amati : “ Khulupilila Yehova ndi mtima wako wonse , ndipo usadalile luso lako lomvetsa zinthu . ( Maliko 15 : 44 ) Ngati Yosefe analipo pamene Yesu anali kuvutika na ululu pa mtengo wozunzikilapo , mwina zimene anaonazo zinamukhudza kwambili cakuti anaona kuti afunika kudzidziŵikitsa kuti ni wophunzila wa Yesu . Pamene Baraki anali kutsogolela gulu lake ku Phili la Tabori , anakondwela popeza anali ndi wowalimbikitsa . Kukoma mtima kwa Yehova kuli na colinga . ( 2 Akor . Siikamba ciliconse za cikhulupililo ca mwana wa Inoki , Metusela , amene anakhala na moyo wautali pa anthu onse ochulidwa m’Baibo . Metusela anakhala na moyo mpaka m’caka cimene kunacitika cigumula . Zili monga kuti Yehova akuwaitana kuti : “ Bwelelani kwa ine ndipo ine ndibwelela kwa inu . ” Kuganizila zitsanzo za amuna ndi akazi akale amene anayembekezela Yehova moleza mtima kuti adzakwanilitsa malonjezo ake , kungatithandize kuyembekezela na mtima wonse . Iye anaonetsa kuti pokhala okondela ena , iwo anali kuphwanya lamulo lacifumu , limene limati : “ Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . ” Munthu wosamalila maluŵa amakonza bwinobwino nthaka , amaithilila ndi kuika manyowa . Kwa zaka zambili , ndinaphunzila Baibulo ndi anthu oculuka , ndipo 11 mwa io anabatizidwa . Tikaganizila za anthu a m’gawo lathu , timafunitsitsa kuwathandiza kuona zinthu zabwino zimene akuphonya . Mwana wina wa mayiyu anali mnyamata wa zaka 12 , ndipo anali wamanyazi kwambili cakuti anali kukonda kubisala phunzilo lisanayambe . M’kupita kwa nthawi , tinauzidwa kuti tikatumikile kum’mwela kwa London . * — Mac . 6 : 7 ; 12 : 24 ; 19 : 20 . Coyamba , ayenela kuona ngati angakwanitse kuphunzitsa ana awo kukonda Yehova panthawi imodzi - modzi kuwaphunzitsa cinenelo cina . M’zaka zaposacedwapa , anthu a Mulungu akhala akugwilitsila nchito cinenelo pomasulila Baibulo n’colinga cakuti anthu aphunzile za Yehova . Tinali kupatsiwa cakudya ca masana , cimene ine na mkazi wanga tinali kudya tikalibe kubwelela ku nyumba . Kodi a nkhosa zina angacite ciani kuti aike maganizo ao pa zinthu zakumwamba ? 2 : 24 ; Filim . Kodi anali kuyembekezela kuti Yehova adzam’patsa zimene anapempha ? Masiku ano , magulu onse aŵili amatumikila Yehova pamodzi , ndipo ali ndi Mfumu imodzi , Yesu Khiristu . Pa maholide , anali kuyesetsa kuniphunzitsa zimene anali kuphunzila m’Baibo . Kukamba zoona , kukambilana nawo kunali kovuta cifukwa sanali kudziŵa cinenelo camanja . Mfundo ya Yesu pamenepa inali yakuti mmene timagwilitsila nchito cuma cathu , zingaonetse kuti ndise ‘ okhulupilika ’ kwa Mulungu kapena ayi . N’ciani cingathandize mwana wanu kuyamba kutumikila Yehova ? Zimenezi zinali zovuta . Kodi Yesu anaonetsa bwanji khalidwe limeneli ? Nimaona kuti ni mwayi waukulu kukhala mu utumiki wa nthawi zonse kwa zaka zoposa 40 . Nakumana na zambili zokondwetsa na kulandila madalitso oculuka . Iye sanafele mbalame , koma anafela ife anthu kuti tikasangalale na moyo wosatha . — Mat . Nthawi zina zitsulo zimenezo zinali kukhala zokhota ngati cikwakwa . Kodi muganiza kuti n’ciani cikanacitikila asilikali ngati mamvekedwe a lipenga sanadziŵike bwino ? Khalani osamala kuti musamangidwe m’goli ndi osakhulupilila ( Onani palagilafu 10 ) Mwana wa sukuluyo anasamukila ku Côte d’Ivoire . Komabe , monga mmene Gayo anacitila , ifenso tingathandize ndi kulimbikitsa Akhristu amene amayenda - yenda , monga oyang’anila dela na akazi awo . Cifukwa Cake Tifunika Kukhala Oyela , 11 / 15 9 , 10 . ( a ) Kodi adani a Yesu anamuyesa bwanji kuti atengeko mbali m’mikangano ya ndale ? ( Machitidwe 17 : 26 , 27 ; Salimo 145 : 18 . ) Tamuuzani kuti andithandize . ” ENA AMAKAMBA KUTI IYAYI . Nikaganizila za umoyo wanga wakale , nimakondwela cifukwa Baibo yanithandiza kudziŵa mmene mwamuna weni - weni afunika kukhalila . [ 1 ] ( ndime 12 ) Ena amene anathetsa mikangano mwamtendele ndi Yakobo , ndi Esau ( Genesis 27 : 41 - 45 ; 33 : 1 - 11 ) ; Yosefe ndi abale ake ( Genesis 45 : 1 - 15 ) ; Gidiyoni ndi a Efuraimu ( Oweruza 8 : 1 - 3 ) . Anatenganso kapu ya vinyo , ndipo atapemphelanso , anawauza kuti : “ Imwani nonsenu . ” Ndipo caciŵili , ndikuyamikilani poyesetsa kufufuza yankho la funso lanu m’Baibulo . Koma pambuyo pake , Rehobowamu anakafunsila malangizo kwa acinyamata anzake . Apa sitikamba za Mkhiristu amene nthawi zina amaganizilako za zakudya , nchito , zosangulutsa , ngakhale zacikondi . Ndinakhumudwa kwambili kuona kuti Mulungu sanayankhe zimene ndinali kufuna . ( Yobu 32 : 5 - 10 ) Yobu atalandila uphungu wa Mulungu ndi kusintha maganizo ake , Yehova anauza anzake a Yobu mau omuyamikila cifukwa ca kukhulupilika kwake pa ciyeso . — Yobu 42 : 7 , 8 . Kucita zimenezi kudzatithandiza kupilila mayeselo pamene tisumika maganizo pa “ ciyembekezo cotsimikizika ” ca Cikhiristu . Kukamba zoona , mau amenewa anali kunikhumudwitsa kwambili . Koma tsopano Iye anali kudzakhala mtumiki wamba wa pa cihema . ( 1 Tim . 3 : 15 ) Mwa ici , timadziŵa kuti Yehova ali na ufulu wotiikila malamulo na kutipatsa cilango mwacikondi ngati taphwanya malamulowo . Koma Baibo imati : “ Mtima wodekha ndiwo moyo wa munthu . ” ( Miy . ( Aroma 14 : 12 ; Agal . 11 : 8 - 10 ) Nthawi zonse , iye anali kudalila Mulungu monga Gwelo la cuma ceni - ceni , ndipo sanali kufuna - funa cuma cakuthupi cifukwa kucita zimenezo kukanaonetsa kuti analibe cikhulupililo . Inunso mukamaŵelenga Mau a Mulungu , mudzalimbikitsidwa kucita zinthu zimene zidzawonjezela cimwemwe canu ndi kulimbitsa ubwenzi wanu ndi Mulungu . Mudzalimbikitsidwanso kuthandiza ena kufuna - funa Mulungu . Ngakhale kuti tsopano n’nayamba kuseŵenza , nimayesetsa kukhala na umoyo wosafuna zambili mogwilizana na malangizo a Yesu a pa Mateyu 6 : 20 - 22 . Kodi mphatso ya Mulungu yopambana zonse imene anatipatsa ni iti ? Kodi ndani akutsogolela pa “ utumiki wokhazikitsanso mtendele ” ? Nanga akucita bwanji utumiki umenewu ? ( Aef . 3 : 8 ) Uthenga umene Paulo anali kulengeza ni umene uli wofunika ngako kuposa maonekedwe ake . Posapita nthawi , amuna atatu alendo , anabwela ku hema wa Abulahamu . Khalidwe limenelo ni nzelu zopindulitsa . Ndipo mumagwilitsila nchito mphatsoyo cifukwa mumaiona kukhala yofunika . Monique wakhala akutumikila ku Myanmar kucokela mu December 2014 . Iye analoŵa m’kacisi kukapeleka nsembe ngakhale kuti sanali wansembe . Acinyamata , mumaonetsa kuti ndinu wolimba mtima pamene mumauza anzanu a kusukulu ndi ena kuti ndinu wa Mboni za Yehova . Peji imene pali mutu wa Baibo ya Ciheberi yomasulidwa na Hutter mu 1587 Coyamba , tiyeni tikambilane zimene wokwela pa hosi aliyense akuimila . Nchito zimenezi ndi “ dama , zinthu zodetsa , khalidwe lotayilila , kupembedza mafano , kucita zamizimu , udani , ndeu , nsanje , kupsa mtima , mikangano , kugaŵikana , magulu ampatuko , kaduka , kumwa mwaucidakwa , mapwando aphokoso , ndi zina zotelo . ” 19 : 3 ) Kusudzula akazi kumeneko Yehova Mulungu anali kudana nako ngako . — Ŵelengani Malaki 2 : 13 - 16 . Pambuyo poŵelenga lembali , tingam’funse kuti : “ Ngati Yesu ndi Mulungu , ndani anam’tuma kubwela padzikoli ? Tikamaceleza anthu amene sangatibwezele zilizonse , timasangalala cifukwa timakondweletsa Atate wathu wakumwamba . — Mateyu 5 : 44 - 46 ; 1 Petulo 4 : 9 . Abulahamu anamuyankha kuti : “ Udzamasuka ku lumbiloli . ” Chulani cifukwa cimodzi cimene Yehova alili woyenela kulamulila dziko . Conco , zolengedwa zonse zimaonetsa kuti Yehova ndiye Mlengi wathu , ndiponso zimaonetsa makhalidwe ake monga mphamvu , nzelu , ndi cikondi . Kwa zaka 7 zimene natumikila kuno , sindinasoŵepo cakudya , ngakhale malo ogona . ” Mboni za Yehova zimakhulupilila kuti mfundo za m’Baibulo n’zopindulitsa . Ndithudi , Yehova amagwilitsila nchito Baibulo kuti atithandize kupilila mavuto paumoyo wathu . ( Luka 6 : 40 ) Kukhala na mtima wokonda kutsatila mfundo za Mulungu ndiye citetezo camphamvu kwa mwana , cifukwa kudzam’thandiza kusagonja potsatila njila zolungama za Yehova . — Yes . Kwambili ! ( Ŵelengani Mateyu 6 : 14 , 15 . ) Iye anatipatsa mwayi wobwelela m’banja la Mulungu . ( Aheberi 13 : 23 ) Ndiponso iye ndi Paulo anali kukonda ndi kudela nkhawa abale ndi alongo ao Acikristu . ( Mlaliki 9 : 10 ) Komabe , Mulungu adzathetselatu imfa mwa kuukitsa akufa . — 1 Akorinto 15 : 26 , 55 ; Chivumbulutso 21 : 4 . Mukapatsidwa zocita , muzivomela mwamsanga ngakhale zioneke kuti ndi zotsika . Yesu atapita kumwamba , kodi atumwi ake ayenela kuti anadzifunsa ciani ? Koma oipa adzacotsedwa padziko lapansi ndipo acinyengo adzazulidwamo . ” 20 : 3 - 5 ) Ngakhale n’conco , iwo anayamba kulambila mwana wa ng’ombe . Koma ena ambili anatengedwa n’kuyamba kusamalidwa ndi abale awo auzimu a m’dzikolo , ndiponso a ku Russia . M’malo mwakuti atumikile Mululungu mwaufulu , io amatumikila anthu amene ali nao ndi nkhongole . ( Yak 1 : 25 ) Iye anakumbukila mmene anaonekela pagalasi ndipo anapitiliza kudzikonza . Mwacitsanzo , pamene wophunzila wina dzina lake Simoni anapempha kuti agule mzimu woyela kwa atumwi , io anakana kulandila ciphuphu ndipo anamuuza kuti : “ Lapa coipa cakoci . ” 4 : 23 , 24 ) Ngati tiyesetsa kukamba na kucita zinthu mogwilizana na cifunilo ca Mulungu , Yehova sadzalola Mdyelekezi kutiwononga kothelatu . — Ŵelengani Salimo 34 : 7 . Gogi akadzayamba kuukila kwake , Yehova adzauza atumiki ake kuti : “ Inu anthu anga , pitani mukaloŵe m’zipinda zanu zamkati ndipo mukatseke zitseko . Mkazi wina wa ku Nigeria dzina lake Joy anavomeleza kuti , “ Ngati sindinagwilizane ndi zimene amuna anga afuna , io amakamba kuti ‘ Ufunika kucita zilizonse zimene ndakamba cifukwa ndine mwamuna wako . ’ ” Mofanana ndi zimenezi , Mlengi wathu watipatsa malamulo amene angatiteteze ku zotulukapo zoipa za ucimo na kutithandiza kukhala na umoyo wabwino . “ Ngakhale masomphenyawa atazengeleza , uziwayembekezelabe . ” — HAB . ( Aheb . 7 : 24 , 25 ) M’nthawi yakale , zimene mkulu wa ansembe anali kucita zinali kuthandiza Aisiraeli kutsimikizila kuti macimo awo akhululukidwa . Mofanana ndi Yesu , anthu ambili masiku ano amalimbikitsidwa akaona mmene Mulungu wawathandizila kusankha zinthu mwanzelu . Nawonso ni anthu a Yehova . Yoswa caputa 2 , 6 ; onaninso Aheberi 11 : 30 , 31 ; Yakobo 2 : 24 - 26 “ Kosi imeneyi inali yaulele ndipo inali yosangalatsa kwambili ” — Aimé , Benin . Mwina tingafunse kuti : Kodi “ mapeto a nthawi ino ” satanthauza nthawi yamtsogolo imene zinthu padzikoli zidzaipa kwambili ? Mipingo ya zinenelo zina kapena tumagulu ingapindule kwambili ndi citsanzo ca abale ndi alongo acikulile . Mwina Yosiya anaphunzitsidwa za cifundo ca Mulungu ndi Mfumu Manase italapa . 5 : 28 , 29 ) Mukaganizila ciyembekezo cokhala ndi moyo padziko lapansi mumayamikila kwambili Yehova . Angacite zimenezi mwa kukhala citsanzo cabwino kwa iwo ndi kuwalangiza mwacikondi . Patapita zaka zocepa , a Bob Atkinson anafika panyumba pathu , ndipo anatenga galamafoni yawo n’kutilizila imodzi mwa nkhani zojambulidwa za M’bale Rutherford . ( 1 Akorinto 10 : 6 - 11 ) Tiyenela kucita zilizonse zimene tingathe kuti tipewe kutengela maganizo a dzikoli . Iye anati : “ Nimayamikila ngako kuti Yehova ananionetsa cifundo cacikulu na kunikhululukila . ” Ine n’nali mtsikana wa zaka pafupi - fupi 19 wocokela ku tauni , koma iye anali na zaka 25 ndipo anali wocokela ku mudzi . Anatiuza kuti tizicita misonkhano yonse mlungu uliwonse ngakhale kupezeke anthu ocepa . Zimenezi zinandithandiza kuti ndikhale ndi maganizo oyamba upainiya wa nthawi zonse ” . Titangofika kumeneko , msilikali wina wa gululo anatilamula kuti tipite ndi kagulu ka zigaŵenga kukamenya nkhondo . * ( Ŵelengani 1 Atesalonika 4 : 3 - 8 ) Yehova ali na ufulu wotipatsa malamulo cifukwa ndiye anatilenga . Tingadziŵe bwanji kuti sitikonda zosangalatsa mopambanitsa ? Yehova Mulungu Amakonda Kukamba ndi Anthu 17 , 18 . ( a ) Ni mphatso yanji imene lemba la Yohane 15 : 16 limachula ? ( Onani pikica kuciyambi . ) ( b ) N’cifukwa ciani mahosi a m’masomphenyawo anali a mitundu yosiyana - siyana ? Janet amagwilitsila nchito mfundo ya m’Baibulo mwa kupewa kudzipatula kuti acepetseko nkhawa zake . Mukabwele ku misonkhano yathu , sitilipilitsa . * Conco , iye anaganiza zomasulila yekha Baibo ya Cipangano Catsopano kucoka m’Cigiriki kupita m’Ciheberi . Kodi anacita mwadala , kapena panali zifukwa zomveka , monga zinthu zosayembekezeleka kapena zakugwa mwadzidzidzi zimene zinapangitsa kuti asacitile mwina koma kukhala m’nyumba imodzi usiku wonse ? ( Mlal . Lemba la Chivumbulutso 19 : 9 limati : “ Odala ndiwo amene aitanidwa ku phwando la cakudya camadzulo la ukwati wa Mwanawankhosa . ” 1 : 11 ; Yak . 1 : 3 , 4 ) Komanso , kuleza mtima kumaphatikizapo kulolela kuvutika popanda kubwezela , ndi kukhala wolimba ndi wosagwedezeka m’cikhulupililo olo tikumane na mavuto otani . Ŵelengani Aefeso 1 : 7 . ▪ Mulungu adzapulumutsa anthu amene amawayanja ndipo io adzasangalala padziko lapansi . M’nthawi za Baibulo Kunali Nsalu za Mitundu , Na . 41 : 10 - 13 . Yesu Kristu anali Mphunzitsi wamkulu woposa onse amene anakhalapo padziko lapansi . Iye analinso mnzao wapamtima . Ine na mkazi wanga tinapeleka mapemphelo ambili mocokela pansi pa mtima . Acicepele athu ambili amacita zimenezi ku sukulu , ndipo sacita manyazi kapena kuopa . N’ciani cikuonetsa kuti Yesu anali wacifundo ? N’kutheka kuti Jowana analinso pakati pa ophunzila a Yesu amene anasonkhana ku Yerusalemu pa Pentecosite mu 33 C.E . Anthu enanso amene ayenela kuti anali pakati pao anali amai ake a Yesu ndi abale ake . ( Mac . Makhalidwe amenewa ni ofunika kwambili kwa anthu otsogolela pa kulambila koona . ( a ) Kodi Yesu anathandiza bwanji ophunzila ake kuona kufunika kwa Ufumu wa Mulungu ? Pa sekondi iliyonse , dzuŵa limatulutsa kuwala ndi kutentha kwakukulu . Koma ndi mphamvu yocepa cabe yocoka ku dzuŵa imene imafunika kuti zamoyo zikhalepo pano padziko lapansi . Ndimayamikila Mulungu kuti panthawi yonseyi , banja langa silinagonepo ndi njala . ” Conco , Paulo anacilitsa mwamunayo mozizwitsa . — Machitidwe 14 : 5 - 10 . Anatelo Janet . Janet anapeza nchito , koma ndalama zimene anali kulandila sizinali zokwanila kusamala banja lake . Kumeneko , anakhazikitsa mipingo yacikhristu pakati pa anthu amene sanali Ayuda . 13 : 57 ; Maliko 6 : 4 ; Luka 4 : 24 ; Yoh . 2 : 10 - 12 ; 1 Pet . Comvetsa cisoni n’cakuti n’nali kucitanso zaciwelewele . Pamene tinali ku Tallinn , Maria anabeleka mwana wathanzi wamwamuna dzina lake Vitaly . Koneliyo asanabatizike monga Mkhiristu woyamba wosadulidwa wakunja , mngelo anam’tsogolela kuitana mtumwi Petulo . Nditafika zaka 10 , atate anamwalila cifukwa ca kumwa moŵa kwambili . ( Yesaya 60 : 22 ) N’zoonekelatu kuti ulosi umenewu ukukwanilitsika masiku ano . Yehova akapeleka thandizo , ubwenzi wanu ndi iye umalimba kwambili . Ndine wokondwela kwambili . ” — Karen . Merten ) , Na . Iye anali kukonzela Yesu cakudya capadela , ndi kucita zinthu zambili kuti maceza ao akhale osangalatsa . N’cifukwa ciani cikhulupililo na cikondi n’zofunika ? Kuti mudziŵe mmene mungacitile zimenezi , pemphani wa Mboni za Yehova kapena yendani pa webusaiti yathu ya www.jw.org . Mulungu nthawi zambili wakhala akuteteza abale athu amene akhala okhulupilika mwa kusatenga mbali m’zandale . Amene amagwilitsila nchito pelefyumu mosapitilila malile sayenela kudziona kuti ndi olakwa . ( 1 Timoteyo 1 : 3 ; 4 : 6 , 7 , 11 , 12 ) Paulo anam’patsanso malangizo othandiza okhudza matenda ake a m’mimba amene anali kumuvutitsa . — 1 Timoteyo 5 : 23 . Kodi Yesu Anali Kuoneka Bwanji Kweni - kweni ? 23 : 8 - 12 . Pita ukayanjane ndi m’bale wako coyamba , ndipo ukabwelako , peleka mphatso yako . Tiyeni tikambilane zifukwa zake . Izi zingaonetse kuti iwo saona kufunika kokhala na zolinga zauzimu . Koma inu simufunika kucita zimenezo cifukwa Baibo imati : “ Maso a Yehova akuyendayenda padziko lonse lapansi kuti aonetse mphamvu zake kwa anthu amene mtima wawo uli wathunthu kwa iye . ” Tiyeni tipende zitsanzo zina za makhalidwe amenewo . — Ŵelengani 2 Timoteyo 3 : 1 , 13 . Mtumwi Petulo ayenela kuti anali ndi zaka zoposa 50 pamene anapita kumalo osoŵa . Kumeneko n’nakumana ndi mlongo wina wodzipeleka potumikila Mulungu , dzina lake Claudia , ndipo tinamanga banja mu 1999 . Mlongo wina analembela mlendo amene anakamba nkhani kuti : “ Olo kuti tinakambilana kwa mphindi zocepa cabe , munanitonthoza na kunitsitsimula monga kuti munali kudziŵa bwino cisoni conse cinali mumtima mwanga . Kodi kuona zinthu mmene Yehova amazionela kumabweletsa madalitso otani ? Lili ndi nkhani zokhudza Mulungu , Yesu Kristu , kuvutika kwa anthu , ciukililo , pemphelo , ndi zina zambili . N’nali kufuna kukondweletsa Mulungu cifukwa coopa kuŵeluzidwa ndi kutenthedwa kumoto wa helo . ( a ) Malinga n’zimene takambilana , kodi Yesu anali munthu wotani ? Mtumwi Petulo anakamba za cikhulupililo cimene “ cayesedwa . ” ( b ) N’cifukwa ciani Akristu a zaka za m’ma 50 kapena kuposelapo ayenelanso kucita cidwi ndi uphungu wa Solomo ? Umoyo unali wovuta . Atabwelela ku nyumba , anapempha kuti ayambe kuphunzila Baibo kaŵili pa wiki . Mwacitsanzo , ndinali kugula zinthu zambili zopakidwa golide mwacinyengo monga mphete , zibangili , ndolo kapena kuti masikiyo n’kuzidinda mau akuti golide wolemela magalamu 2.8 . Ndipo zinthu zimenezi ndinali kuzigulitsila m’malo oimikapo magalimoto pa masitolo akuluakulu . Ndiponso pamene Yehova apeleka malangizo kwa ana ake odzozedwa kupyolela m’Mau ake , mzimu woyela umakulimbikitsani kutsatila malangizowo , ndipo mumtima mwanu mumati , “ Malangizo amenewa agwila nchito kwa ine . ” ( Yohane 11 : 25 ) Ndithudi , Yesu ali ndi mphamvu zoukitsa akufa kuti akhalenso ndi moyo . Nthawi zina sitingamvetsetse cifukwa cake tapatsidwa nchito zatsopano . ( Miyambo 11 : 25 ) Nanga mungathandize bwanji anthu a m’gawo lanu ? Kudziŵa kuti munthu amene timakonda adzamwalila kumavutitsa maganizo . N’ciani cinacititsa Davide kuyamikila mkaziyu ? Nanga citsanzo ca mkazi ameneyu citiphunzitsa ciani ? Koma sitinacite zimenezo mwa kumamatila Cilamulo ca Mose , kapena mwa kucita zinthu zina kuti Yehova atiyanje iyai . M’bale Peter atafunsidwa kuti anamva bwanji na masinthidwe amenewo , anayankha kuti : “ Ndine wokondwa ndi wonyadila kuti pali abale amene anaphunzitsidwa kutenga maudindo aakulu , amenenso akuwasamalila bwino ngako . ” Koma Samueli anayesetsa kukonzekeletsa mtima wa Sauli pang’onopang’ono . Pamene tiyanjana ndi abale na alongo athu , timapeza mabwenzi eni - eni komanso apamtima . Kodi Irina wapindula bwanji cifukwa coganizila zinthu zabwino zimene ali nazo ? ( Danieli 2 : 44 ) Umphawi , matenda , ndi imfa sizidzakhalakonso . Ndiyeno mudzakwanitsa kuwapatsa mphatso imene adzakondwela nayo . N’cifukwa ciani tiyenela kukhala okhulupilika ndi oona mtima polambila Yehova ? Mukangoona mwalawo simungazindikile kuti muli golide . Sizingatheke kuti muzidya patebulo la Yehova komanso patebulo la ziwanda . ” — 1 Akor . Mungacite izi : Muziŵelenga na maganizo oyenela , muziona mfundo zimene mungaseŵenzetse ; muzidzifunsa mafunso monga akuti ‘ Kodi mfundo izi ningaziseŵenzetse bwanji pothandiza ena ? ’ Pambuyo pake , mpingo wacikristu unayamba kutsatila “ cilamulo ca Kristu . ” Tsiku lina atafika m’nyumba , anapeza kuti wapolisiyo wagona pabedi yake . Kodi tingakonzekele bwanji cocitika cimeneci ? Kodi tidzapindula bwanji tikadzapezekapo ? Nanga Cikumbutso cimagwilizanitsa bwanji anthu a Mulungu pa dziko lonse ? Mtsikana akuuzako anzake a kusukulu uthenga wabwino ndi kuwapatsa kapepala ka uthenga . N’tacoka ku msonkhano , n’nali n’tatsimikiza mtima kukhala wolimba m’cikhulupililo ku sukulu . Lamulo loyamba linali lokhudza nchito yolalikila . Koma kodi Yehova anacita ciani ? Phunzilani Malemba amene adzakuthandizani kukana kutenga mbali m’ndale ndiponso amene amakamba za madalitso a m’dziko latsopano Kodi Yehova amapulumutsa bwanji anthu ake ? ( 1 Tim . 3 : 4 , 5 ) Bungwe la akulu pamodzi na wadela amapenda bwino - bwino ziyeneletso za m’Malemba za akulu ndi atumiki othandiza . — 1 Tim . 5 : 3 ) Kuwonjezela apo , kumvetsetsa bwino mfundo za coonadi ca Mau a Mulungu , kudzatithandiza kukhala wokonzeka kuteteza molimba mtima coonadi kwa otsutsa . — 1 Pet . Afunika cilango cowakhaulitsa mokwana ! ” Kucita zimenezi kunali ngati cakudya canga . Mwinanso mungaganize kuti kuuza akulu za chimolo kuti am’thandize , kungaoneke ngati kusakhulupilika kwa mnzanuyo . Tingawathandize bwanji acicepele kapena obatizika catsopano kupita patsogolo ? Palibe nchito ina imene ingatipatse cimwemwe ceni - ceni kuposa imeneyi . Koma mfundo ndi yakuti cikhulupililo cimeneci sicimapeleka ciyembekezo ciliconse cakuti mavuto adzatha . Anthuwo analibe ndalama zogulila Mabaibulo kuchalichi kwao , ndipo nthawi zambili sanali kumvetsa tanthauzo la mavesi ena m’Mabaibulowo . ” Iye sapangitsanso zinthu zoipa kucitika kapena kulimbikitsa ena kucita zinthu zoipa . 10 : 21 . Iye anati : “ Pamene tinakuka , mkazi wanga anati , ‘ Anzanga onse anatsala mu mpingo wathu wakale . ’ ” 8 : 29 ; 14 : 9 ; 15 : 10 ) Mwacitsanzo , ganizilani mmene mneneli Yesaya anafotokozela cifundo ca Yehova . Kudzilanga tekha kumatithandiza kukwanilitsa zolinga zauzimu . Tizionetsa kuti timayamikila akulu mumpingo . ( Mac . N’zosakaikitsa . Malinga n’zimene Yearbook ya 1944 inakamba , msonkhanowu “ unacititsa kuti Mboni za Yehova zidziŵike kwambili ku Mexico . ” N’ciani cinacititsa kuti asinthe maganizo ? Magaziniyo inalibe zinthuzi zilizonse , ndipo makope 6,000 ndi amene anasindikizidwa . ( Aheberi 6 : 18 ) Zoona zake n’zakuti Satana ndiye anakamba bodza pamene anauza Hava kuti : “ Kufa simudzafa ayi . ” — Genesis 3 : 4 . Satana amaseŵenzetsa dzikoli kuti atipangitse kuganiza kuti tingakhale acimwemwe pokhapo ngati tili ndi zinthu zambili . Wosimba ndi Yvonne Quarrie M’kupita kwa nthawi , tingayambe kucita zinthu zoipa zimene poyamba sitinali kuganiza kuti tingazicite . Ni mfundo yofunika iti imene sitiyenela kuiiŵala ? 9 , 10 . Gulu loukilalo linacita mantha n’kuthawa . Iye analonjezapo Abulahamu kuti azamupatsa mwana , koma Abulahamu anafunika kuonetsa cikhulupililo na kuleza mtima . Christopher Mavor “ Cikhulupililo ndico . . . umboni wooneka wa zinthu zenizeni , ngakhale kuti n’zosaoneka . ” — AHEB . Pa zaka 100 zapitazi anthu mamiliyoni ambili anafa cifukwa ca nkhondo makamaka pa nkhondo ziŵili za padziko lonse lapansi . Zimandikhudzabe ndikaona anthu akuvutika ndi nkhanza . Nanga ndi zinthu ziti zimene tiyenela kusamala nazo ? Timam’khulupilila kuti adzadalitsa khalidwe lathu , ndipo madalitso ake ndi ofunika kwambili kwa ife kuposa kubwezela zoipa zimene ena anaticitila . Masiku ano , cisautso cacikulu cisanayambe , tilinso ndi mipata yambili yoonetsela cikondi kwa abale athu . MUNGAYANKHE bwanji munthu atakufunsani kuti , ‘ Kodi ziphunzitso zofunika ngako pa cikhulupililo canu n’ziti ? ’ Mwakabisila , mlonda wa ndendeyo anatiuza kuti : “ Sikuti boma limakuzondani . Kodi okwatilana angalole motani Yehova kutsogolela banja lao ? 4 Kukhulupilila Nyenyezi Komanso Kulosela Zakutsogolo — Kodi N’kodalilika ? Kodi angelo aliko zoona ? Conco pamenepa ndi pomwe timadziŵila kuti ulosiwu sukamba za Nebukadinezara cabe . Conco , tingawathandize bwanji kuti apite patsogolo ? Gidiyoni anadziona kuti sanali ‘ wamphamvu ’ ndi kuti sakanakwanitsa kulanditsa anthu a Mulungu . Kodi tingapeleke bwanji citonthozo ngati taona kuti n’zovuta kukamba na munthu pamaso - m’pamaso ? ( Mat . 25 : 31 - 33 ) Kodi nkhosa ndi mbuzi zidzapatsidwa ciweluzo cotani ? Koma naonso amene alandila uthengawo amaona kuti nthawi ndi ya mtengo wapatali . ( Miyambo 7 : 7 ) Ngati mwaona kuti nkhani inayake ndi yovuta kukhulupilila , ndiye kuti mwina nkhaniyo ndi yabodza . Kodi mau amenewa si okhazika mtima pansi ? Paulo anakamba kuti Kristu “ wapelekedwa monga nsembe yathu ya pasika . ” — 1 Akor . Mose anafunsa Aisiraeli funso ili : “ Ndi mtundu winanso uti wamphamvu umene uli ndi malangizo ndi zigamulo zolungama zofanana ndi cilamulo conseci cimene ndikukuikilani pamaso panu lelo ? ” Atate sanasangalale ndi zimenezi cakuti anasiya kukamba nane ndipo anayamba kundipewa . Pamene ndinali kuphunzila Baibulo ndinaona kuti ndifunika kusintha zinthu zambili . Nthawi zina , timakhala otopa pamene ticoka pa nyumba kupita kumisonkhano kapena mu ulaliki . Zimenezi zimakulimbikitsani cakuti mumayamikila kwambili nkhani imeneyo . Pambuyo pakuti Samueli ndi Sauli adyela pamodzi cakudya cokoma , kuyendela pamodzi , kuceza , ndi kupuma , Samueli anaona kuti tsopano inali nthawi yabwino yakuti adzoze Sauli . Kodi mungacule ubwenzi wanu wamtengo wapatali ndi Yehova ? Cikondi sicicita nsanje , sicidzitama , sicidzikuza , sicicita zosayenela , sicisamala zofuna zake zokha , sicikwiya . ( Mat . 23 : 8 ) Amuna a maudindo mumpingo anatengeka kwambili na ziphunzitso za Aristotle ndi Plato . 20 : 1 - 3 , 6 ; 21 : 3 , 4 . Maonekedwe athu amakamba zambili za ife . Kodi mkulu angakonzekeletse bwanji mtima wa wophunzila ? Nanga n’cifukwa ciani kucita zimenezo n’kofunika kwambili ? Umoyo Wosalila Zambili Umabweletsa Cimwemwe , May 17 : 6 ) Patapita zaka zambili , Ababulo anagonjetsa Asuri . Conco panthawi imeneyo , Aisiraeli ambili amene anatengedwa ukapolo anali atamwazikana mu ufumu wonse wa Babulo . Kutalitali ! Mtumwi Petulo anatengela Yesu pambali ndi kumuuza kuti : “ Dzikomeleni mtima Ambuye . Ine ndisanakhaleko kunalibe Mulungu amene anapangidwa , ndipo pambuyo panga palibenso wina . Malinga n’zimene lemba la Chivumbulutso 5 : 13 limakamba , “ wokhala pampando wacifumu , ndi Mwanawankhosa ” afunikadi kulemekezedwa . Panthawiyo , nkhaniyi inali yovutitsa maganizo kwambili . N’cifukwa cake , tiyenela kulemekeza ufulu wao wosankha nthawi yakuti afalitse nkhaniyo , ndi mmene angaifalitsile . 5 : 19 ; Yoh . 8 : 44 ) Tsopano , Satana wakhala katswili ‘ wocititsa khungu maganizo a anthu ’ cakuti “ akusoceletsa dziko lonse lapansi kumene kuli anthu . ” ( 2 Akor . 4 : 4 ; Chiv . Ndithudi , wakhala mwayi wamtengo wapatali kuyenda m’maiko oposa 90 , mu utumiki umenewu . Pamene anali kukambilana , Janet mosamala anapempha mlongoyo kuti amasuke na kufotokoza cimene cinam’khumudwitsa . ZAKA zoposa 3,000 zapita , Yobu wa m’nthawi yakale anazindikila kuti mbalame za m’mlenga - lenga zingatiphunzitse zambili ponena za nchito za Mulungu . Ndiyeno woyang’anila msonkhanowo anati : “ Alekeni apite ! ” Koma mzimu woyela unamuthandiza kusintha . Nkhawa zinanikulila kwambili . Nkhani imeneyi idzafotokozedwa bwino m’nkhani zina za kutsogolo pa mbali yakuti “ Za m’Nkhokwe Yathu . ” — Za m’nkhokwe yathu ku Central Europe . Nili na amayi , ndipo pambuyo pake nili na atate Zekariya anaona mpukutu ukuuluka mumlengalenga . Mpukutuwo unali wa mamita 9 m’litali na mamita 4.5 m’lifupi . 16 Muganiza Bwanji ? ( Yos . 2 : 9 - 11 ) Cifukwa cakuti Rahabi anagwilizana ndi gulu la Yehova panthawiyo , iye ndi banja lake anapulumutsidwa pamene Aisiraeli anagonjetsa Yeriko . ( Yos . ( Ŵelengani 1 Timoteyo 5 : 2 . ) Ndiye cifukwa cake mabanja ena amacita kulambila kwa pabanja kuciyambi kwa mlungu . Iye anakamba kuti nthawi zina anali kudziona monga munthu “ wotayika ndi wosoŵa anzake . ” Baibo imatilimbikitsa kuti sitiyenela kukayika - kayika kapena kulephela kupanga zosankha . Mwacitsanzo , Aisiraeli anauzidwa kuti : “ Usabwezele coipa kapena kusungila cakukhosi anthu amtundu wako . Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha . Mungafunse ofesi ya nthambi m’dziko lanu kuti mudziŵe mmene mungacitile zimenezi . Kodi mtumwi Yohane anatilimbikitsa kuti tiziganizila za ciani ? Sudziŵa kuti anthu amacoka kuno kupita kumene wacokelako kukafuna nchito ? ” Kodi Nowa anadziŵa bwanji colinga ca Mulungu kwa anthu ? Mosakaikila inuyo mudziŵa kuti m’Baibulo muli uthenga umene Mulungu analembela anthu onse . 13 , 14 . ( a ) Tingaphunzile ciani pa zitsanzo zamakono za anthu okonda zinthu zauzimu ? 16 : 13 - 15 ) Tengelani citsanzo cake . Motelo , ngakhale mwakhumudwa , muyenela kuyesetsa kulankhula mokoma mtima . Tikamamvela lamulo limeneli , Yehova adzatipatsa moyo wosatha Akuluwo anakumbukila kuti pamene woyang’anila dela anabwela ulendo wapita anawalimbikitsa kuti ayeyesetse kuphunzitsa ena . Ganizilani kuti munalipo pamene Paulo anakamba zokhudza ‘ Mulungu amene anapanga dzikoli ndi zinthu zonse zili mmenemo , ’ amenenso “ sakhala mu akacisi opangidwa ndi manja . ” Lembali limati : “ Musabwezele coipa pa coipa . . . . Iwo amagwilitsila nchito mfundo zopezeka m’magazini athu . Okwatilanawo safunika kulola aliyense , ngakhale a dokota , kuwapangila cosankha pa nkhaniyi . Patapita zaka zambili , nthawi inakwana yoti Yehova akonze zinthu kudzela mwa Yesu Kristu , Mfumu yatsopano imene iye anaika . Copambana zonse n’cakuti panalinso “ mtengo wa moyo pakati pa mundawo . ” — Genesis 2 : 8 , 9 . 20 : 1 - 3 . Sitikayikila kuti Yehova anali kutilimbikitsa kupitila m’mauthenga ambili olimbikitsa amene Akhiristu anzathu anali kutitumila . ” Popeza limeneli ndi lamulo kwa alambili onse oona a Yehova , kumvetsetsa buku la Levitiko kudzatithandiza kukhala oyela . Kaamba ka ici , iwo anapempha kuti Mulungu asakambe nawo mwacindunji , koma kuti Mose aziwauza zilizonse zimene Mulunguyo adzakamba naye pa Phili la Sinai . Komanso , ganizilani za mlongo wina wa ku England , amene anali kufunitsitsa kukhala na mwana koma sizinatheke . Conco , m’pomveka kukamba kuti pamene pali Yehova , komanso “ pamene pali mzimu wa Yehova , ” pali ufulu . 6 : 26 , 28 ) Kucita zimenezi kudzawonjezela cidziŵitso canu , mudzamukonda kwambili Yehova , ndipo mudzakhala okonzeka kuphunzitsa bwino ana anu . — Luka 6 : 40 . Tidzafunika kusonyeza makhalidwe amene Yehova akutiphunzitsa tsopano . ( Ŵelengani Yesaya 60 : 17 . ) ( Mac . 15 : 7 ) Pambuyo pa msonkhanowo , Petulo anapita kukakhala ku Babulo . Mosakaikila colinga cake cinali kukalalikila Ayuda ambili amene anali kukhala mumzindawo . ( Agal . Kodi kukhala okhutila kungatithandize bwanji kukonda abale athu ? M’malo mokambilana ndi ana anu kwa nthawi yaitali pamene io safuna , ndi bwino kukambilana nao monga mukuceza . ( Deut . Komabe , palibe buku ina imene yafufuzidwa kwambili ndi kutsutsidwa kuposa Baibulo . Ndi mmenenso zinalili ndi ana a Mfumu Yosiya . Onani mau a munsi aciŵili pa lemba la Ezekieli 18 : 4 ndi Zakumapeto 3B mu Reference Bible . “ Amuna ena m’dzikoli ndi okoma mtima , acikondi ndi acifundo . Mwina zimene mwaphunzila m’nkhani ziŵilizi ponena za buku la Levitiko , zakulimbikitsani kufuna kuphunzila zambili m’Malemba . Yehova anati Mfumu Davide anali “ munthu wapamtima [ pake ] . ” ( Mac . Mu 1944 , pa Nkhondo Yaciŵili Yapadziko Lonse , ndinalamulidwa kuti ndiloŵe usilikali . Nthawi zonse tikacita zimenezi , timakhala osangalala ngako , ndipo koposa zonse , timalimbikitsidwa mwauzimu . Pamapeto pake , io anaonongedwa . ( Mat . 26 : 39 ) Pamene ayenda kukabatizika , ophunzila atsopano amenewo amaonetsa kuti anadzikana okha na kuti ni otsimikiza mtima kutumikila Mulungu na mphamvu zawo zonse , cuma , na maluso awo . Iwo anapatsidwa zimene anali kufunikila . — Aef . M’malo mocita lendi maholo aakulu , nthawi zambili Ophunzila Baibulo anali kupeza malo aulele monga makalasi a pa sukulu , maholo a kumakhoti , masitesheni a sitima , ndi zipinda zocitilamo maseŵela za m’ma nyumba aakulu . Conco , nchito yake imakhala yopanda phindu mofanana ndi “ kuthamangitsa mphepo . ” Iye anati : “ Ndikunena zoona mwa Khristu . . . ndili ndi cisoni cacikulu ndipo mtima ukundipweteka nthawi zonse . ” Kuphunzitsa ana mfundo za makhalidwe abwino 11 : 2 . N’zoona kuti masiku ano si Akhristu onse mumpingo amene amayenda mtunda utali kukalalikila uthenga wabwino . Iye anakulila m’banja lacifumu ndipo “ anaphunzila nzelu zonse za Aiguputo . ” Kodi olengeza Ufumu akwanitsa bwanji kupitiliza kulalikila mosasamala kanthu za kuukila kwa Satana ? Kunena mwacidule , cinawathandiza ndi mfundo za m’Baibulo zimene amagwilitsila nchito pa umoyo wao . Yehova safuna kuti tizimumvela mwamwambo cabe , mokakamizika kapena cifukwa coopa cilango . Mofananamo , si canzelu kuloŵa “ m’cithaphwi ca makhalidwe oipa ” a m’dzikoli n’colinga cakuti mudziŵe kupweteka kwake . — 1 Petulo 4 : 4 . Ngati anthu ena atinena , cingakhale covuta kunyalanyaza zokamba zao . Koma Debora ndi Baraki anali kum’dziwa bwino . M’nyimbo yao , io anauzilidwa kutamanda Yaeli monga “ wodalitsika pakati pa akazi onse ” cifukwa ca kulimba mtima kwake . Kodi mbadwa za Abulahamu zinaculuka motani ? Kodi cikondi cimakwilila bwanji “ macimo oculuka ” ? N’ciani cinapangitsa kuti umoyo wake usinthe kwambili conco ? M’malo moseŵenzetsa mau ambili ovuta kumvetsetsa , Baibulo lili ndi mau amene timawadziŵa bwino . Kodi Mkristu wokhulupilika amene wacibale wake ndi wocotsedwa , ayenela kukhulupilila ciani ? Ndiye cifukwa cake timakondwela kuuzako ena zimene timakhulupilila ndi ciyembembekezo cabwino cimene tili naco . Baibo imafotokoza kuti Atate wathu wakumwamba , Yehova Mulungu amatikonda kwambili ndipo amatiuza zimene iye amafuna kuti ise tizicita . Koma anali wosadziŵa zinthu ndi wopanda nzelu . Ndipo kwa zaka zambili anali kuphunzila zokhudza dzuŵa . N’ciani cinathandiza Yosefe kukhalabe wokhulupilika atakumana ndi ciyeso cimeneco ? N’nafeluka mayeso otsiliza pa sukulu . Ndiponso n’nayamba kucita magesicha na mendo pokamba na anthu . Panthawiyo tinalibe magetsi . Izi zikadzacitika , pa dziko lapansi padzakhala olambila oona a Mulungu okha - okha . Panthawiyo , kulambila koona kudzabwezeletsedwa kothelatu . Amene anali pulezidenti wa dziko la U.S . anati : “ Kucenjeza anthu kukali nthawi . . . kumapulumutsa moyo . ” Nditakhala ndi zaka 10 , ndinali nditayamba kale kuba . 29 : 5 ) Kuyamikila munthu koma tikakhala kuseli n’kumamunena , ni cinyengo . Yehova ayenela kuti anacotsa moyo wa Inoki pang’no - pang’ono kuti asaphedwe mwankhanza ndi adani ake . Mungamvele monga mmene munthu angamvelele ngati waseŵenza kwa moyo wake wonse n’kudziunjikila vindalama , koma pambuyo pake n’kuzindikila kuti ndalamazo n’zabodza . ( Miy . Pambuyo pophunzitsa kosi imeneyi kwa zaka zitatu na hafu , anatiuza kuti tibwelele ku Malawi kuti tikalembe zokumana nazo za Mboni zimene zinazunzidwa cifukwa cosatengako mbali m’nkhondo . ( Machitidwe 8 : 30 , 31 , 34 ) Mofanana ndi nduna imeneyi , inunso ngati mufuna kudziŵa zambili zokhudza Baibo , tikupemphani kuti mutumize pempho lanu pa webusaiti ya www.jw.org kapena mulembele pa iliyonse ya maadresi amene ali m’magazini ino . Zovala zathu ziyenelanso kulemekeza uthenga umene timalalikila , ndi kupeleka ulemelelo kwa Yehova . ( Aroma 13 : 8 - 10 ) Tizivala bwino maka - maka pamene ticita zinthu zauzimu monga kusonkhana ndi kulalikila . 7 , 8 . ( a ) Ni zitsanzo ziti za m’Baibo zimene zionetsa kuti Yehova amafuna kuti tizilimbikitsana ? Komabe , Baibulo limaticenjeza kuti : “ Munthu amene sadziŵa zinthu amakhulupilila mau alionse , koma wocenjela amaganizila za mmene akuyendela . ” — Miyambo 14 : 15 . Zimenezi zitanthauza kuti kutsatila ziphunzitso za Yesu kuyenela kukhala patsogolo paumoyo wathu . Poyembekezela nkhosa , Davide anali kuimba zeze ndi kuona zinthu zokongola zimene Mulungu analenga . ( 2 ) N’zitsanzo ziti zimene zingatithandize kukula mwauzimu ? Iwo anali odzicepetsa , osati odzitukumula . ( Mat . Atapita kucipinda cake , anapemphela kwa Yehova kuti am’thandize . Tsiku lina , atate ake John anam’tuma kuti akapeleke kalata kwa m’bale wina wa mumpingo mwawo . Iye anati : “ Ndinakhala wosungulumwa ndipo ndinali kungokhalila kulila . Ndipo ngati pakhomopo pali munthu wokonda mtendele , mtendele wanu udzakhala pa iye . Ngati n’conco , ndiye kuti mau ake akutiuza zinthu zingapo ponena za amene adzaukitsidwa ku moyo wa kumwamba . Iye analemba kuti m’masiku otsiliza , ana adzakhala osamvela makolo . Mtumwi Petulo anayelekezela Satana ndi “ mkango wobangula . ” Tsopano , tiyeni tikambilane zitsanzo za m’Baibo zimene zimatithandiza kukhulupilila kuti Yehova angathe kutithandiza m’njila imene sitinali kuyembekezela . Zimenezi zinathandiza kwambili cakuti anthu a m’madela onse ozungulila Yuda anayamba kuopa Yehova . Tikamayesetsa kufuna - funa coonadi ngati cuma cobisika , Yehova adzatithandiza kupeza mfundo zatsopano za coonadi zimene tingaike “ mosungilamo cuma ” cathu . 3 , 4 . ( a ) N’ciani cimene Paulo anakamba akalibe kunena mau a pa 2 Akorinto 3 : 17 ? N’ciani cidzacitika nchito yolalikila ikadzatha ? N’ciani cimene Baibulo limakamba ponena za zozizwitsa zimene Akristu a m’nthawi ya atumwi anali kucita ? ( Ŵelengani Yesaya 30 : 21 . ) Koma , ife tinalonjeza Yehova kuti tidzakhala okhulupilika kwa iye . N’cifukwa ciani kulambila Mulungu ku kacisi wa ku Yerusalemu kunali kudzathetsedwa ? Nanga ingatipindulitse bwanji ? KODI MUGANIZA BWANJI ? N’cifukwa ciani Yehova sanalekele cipanduko ? 30 : 19 , 20 . Koma izi sizinawafooketse Ayuda . Iye analemba kuti : “ Pamapeto pake ndinaulula chimo langa kwa inu . Kodi mudzayesetsa kutengela citsanzo ca Yefita ? A Yohane : Zoonadi . Gulu la apaulendo linadutsa mzinda wa Kanani ndi nkhalango yoopsa ya m’dziko la Negebu . Davide anafotokoza kuti : ‘ Yehova adzamucilikiza pamene akudwala pabedi lake . Anthu ena mumpingo agwa ulesi poona kuti akhala akulalikila kwa zaka zambili kuposa mmene anali kuganizila . Tisanayankhe mafunso aya , coyamba tiyeni tione cifukwa cake kusamalila wodwala matenda osacilitsika n’kovuta . 5 : 3 , 6 ; Yoh . 6 : 44 ; 10 : 14 . Kodi makolo angathandize bwanji wacicepele amene wayamba kukayikila zimene amakhulupilila ? Ngati ndinu wacicepele , kodi muli na zolinga zauzimu ? A Yohane : Nanga lembali lionetsa bwanji kuti mbili ya m’Baibulo ndi yoona ? MAFUNSO OCOKELA KWA AŴELENGI . . . Baibulo silimangotiuza kuti tizigwila nchito koma limatiuzanso zimene tiyenela kucita kuti tizisangalala ndi nchito yathu . Kodi tingaphunzile ciani pa kudzicepetsa kwa Gidiyoni ? Lomba pa thebulo yanga nimakhala na ndandanda ya nchito zimene nifunika kucita . Izi ziman’thandiza kucita zinthu pa nthawi yake , osati kuyembekezela mpaka nthawi itatha . ” Koma lomba , timamvela monga ndise a m’banja limodzi , ndipo ndine wokondwa ngako . ” Kodi ndani amene anali mwana woyamba kulengedwa ndi Yehova ? Cofunika kwambili popeleka thandizo kwa anthu othaŵa kwawo si ndalama , koma kupeza nthawi yoceza nawo ndi kucita zinthu zoonetsa kuti timawaganizila . Yesu anali atawalonjeza kuti iye adzakhala nao , ndi kuti mzimu woyela udzawathandiza . Kuzindikila mfundo imeneyi kudzatilimbikitsa kukhala ‘ odzicepetsa pansi pa dzanja lamphamvu la Mulungu . ’ — 1 Pet . Izi zitanthauza kuti makolo muli pa malo abwino kwambili otsogolela ana anu m’njila yoyenela malinga ngati mucita zimene mumawaphunzitsa . N’cifukwa ciani tinganene kuti Kristu anakwela pahachi ‘ cifukwa ca cilungamo ’ ? Kodi webusaiti yodalilika ikutipo ciani pa nkhaniyo ? ’ Kuzungulila dziko lonse , inu acinyamata mumasiyana umunthu , maluso , cidziŵitso , zokonda ndi zimene mumakhulupilila . Atate wathu wakumwamba anaika makonzedwe akuti tizisonkhana nthawi zonse . Colinga n’cakuti tizilimbikitsana wina na mnzake . “ Yehova anagonjetsa Aitiyopiyawo . ” Pamene Mose anali kuganizila kwambili za malonjezo a Yehova kwa Aisiraeli , cikhulupililo cake cinalimba ndipo cikondi cake pa Mulungu cinakula . MLALIKI 4 : 6 Amenewa Yehova amawaonanso kuti ndi ‘ anthu ake osankhidwa mwapadela . ’ — Yes . Yehova ni dzina la Mulungu lopezeka m’Baibo . — Salimo 83 : 18 . Kodi Aisiraeli anakhala bwanji mtundu wa mboni ? Malemba sachula mwacindunji kuti Jowana anali kupeleka ndalama . ( Ŵelengani Ekisodo 14 : 13 , 14 . ) Hachi yotuwa , imene wokwelapo wake akubweletsa imfa mwa kucitsa milili yoopsa . Cenjezo limenelo n’lofunikila ngakhale lelolino . Kodi adzakhala wofunitsitsa kulandila malangizo a Yehova , kapena adzadzipatula mwauzimu ? — Miy . Tili ndi cikhulupililo cakuti Yehova posacedwapa adzayankha pemphelo lathu locokela pansi pamtima lakuti : “ Ufumu wanu ubwele . ” Ponena zam’tsogolo vesi 44 imati : ( Ŵelengani Salimo 24 : 3 , 4 ; Yes . Cina cimene cimatithandiza kukhala na mtendele n’cakuti timayesetsa kukhala pamtendele ndi a m’banja lathu , komanso ndi Akhiristu anzathu mu mpingo . Kodi kumamatila ku miyezo ya Yehova kuli na mapindu anji ? Inde , Yehova wakhala akuonetsa cifundo kwa anthu . Koma maka - maka pamene atumwi onse anafa , anthu ena anayamba kuphunzitsa “ zinthu zopotoka ” kuti “ apatutse ophunzila aziwatsatila . ” ( Mac . 20 : 30 ; 2 Ates . ( b ) Kodi odzozedwa adzadindidwa liti cidindo cao comaliza ? Komabe , mulimonse mmene tapitila patsogolo , tiyeni tipitilize kupita patsogolo mwa kuyenda moyenela m’njila yomweyo . ” ( Afil . Ndipo muzicondelela Yehova kuti akuthandizeni kutsatila mfundo zake pankhaniyi . — Ŵelengani Aroma 12 : 2 . Okwatilana angalimbitse cikwati cao mwa kulankhulana bwino ndi mau “ olimbikitsa monga mmene kungafunikile , kuti asangalatse ” mnzao wa mu cikwati . — Aef . Kapena kodi anaganizila za mwai umene anali nao wokhala kumbali ya Yehova ? 60 : 22 ) Kuposa kale lonse , masiku ano pali anthu ambili amene amakonda Mulungu na anthu anzawo . Mwacitsanzo , kodi amakonda kukamba za mafashoni , ndalama , zipangizo zamakono , zosangalatsa , kapena zolinga zakuthupi ? Mlongo Grace Estep anakamba kuti : “ Nthawi zina , anthu anali kutifunsa kuti , ‘ Kodi khadi limeneli limakamba za ciani ? Tinali kukondwela kukhala pamodzi ndi acibale ndi mabwenzi athu . ” Koma kale Hans sanali wofatsa . Ameneyo ndi Mulungu , wamkulu koposa m’cilengedwe conse . Baibulo limakamba za anthu akale kuti : “ Mosakayikila , iye [ Mulungu ] adzakukomela mtima akadzamva kulila kwako . Mwacitsanzo , timaonetsa kuti timakonda Mulungu ndi anzathu mwa kugwila mwakhama nchito yolalikila uthenga wa Ufumu . Muyenela kupeza nthawi yoganizila cifukwa cake ubatizo ndi wofunika kwambili . Yehova Mulungu wasankha Wolamulila wa dziko lonse wabwino kwambili . “ N’nali kuganiza kuti Baibo ni yovuta kumvetsetsa . ” — Jovy Pambuyo pake , “ anagona limodzi ndi makolo ake , ndipo anaikidwa m’manda mu Mzinda wa Davide . ” ( 1 Maf . ( 1 Akor . 5 : 1 , 2 ) Akristu a ku Korinto akanalekelela chimo lalikulu limenelo , ena mumpingowo akanayamba kutsatila miyambo yonyansa yaciwelewele ya anthu a mumzindawo . Kodi si pake ndithu kuwayamikila madalitso onsewa ? N’napeza nzelu zoculuka kwa iwo cifukwa anali kudziŵa zambili . 27 : 11 ) Mukacita zimenezi , mudzapambana nkhondo yoteteza maganizo anu . ( Ŵelengani Aroma 8 : 14 - 17 . ) Cinsinsi Namba 1 Kukhulupilika Anafika potailatu mtima . Koma atayamba kuphunzila Baibo , anayamba kuona zinthu mosiyana ndipo zinamuthandiza kugonjetsa zizoloŵezi zake zoipa . 5 : 8 , 9 . Lonjezo la Yesu limeneli linazikidwa pa malonjezo a Yehova , amene ni odalilika kuyambila kale . Sitinganene motsimikiza . Mukacita zimenezi , mudzaphunzila zambili . Enanso ni ophunzila kwambili , ndipo ena ni asayansi . Gulu la Yehova padziko lapansi likupita patsogolo m’njila zambili . Yehova atakhazikitsa pangano la mu Edeni , mbeu imeneyi ndiponso mkazi sinadziŵike kwa zaka pafupifupi 4 sauzande . Komabe , Yehova anapanga mapangano angapo otithandiza kudziŵa mbeu imeneyo . Koma anthu onse ocimwa adzafafanizidwa . M’tsogolo , anthu oipa adzaphedwa . ” 43 : 21 ) Iwo anachedwa Mboni za Yehova . Akristu onsewa angaoneke monga kuti ndi ofooka kuuzimu , koma io ndi “ olemela m’cikhulupililo , ” mofanana ndi aja amene angaoneke olimba . — Yak . Akasungidwa , akhoza kuwola ndi cinyontho kapena kudyewa ndi makoswe kapenanso tuzilombo twina , makamaka ciswe ngati amubisa m’nthaka . ” Nthawi zina pambuyo pogwila nchito maola ambili tingadzikakamize kupita ku misonkhano . Mukhoza kupeleka ndalama , zinthu ngati ndolo ( masikiyo ) , mphete , zibangili ndiponso zinthu zina zamtengo wapatali . Ŵelengani Salimo 45 : 3 . Pali zinthu zina zimene tifunika kucita kuti Yehova akhale Bwenzi lathu . Koma nthawi zina kukhulupilila kuti Yehova adzatithandiza kumakhala kovuta . Ngati mukwanilitsa udindo wanu mudzasangala kudziŵa kuti makolo anu akulandila cisamalilo ndi cikondi cimene amafunikila . Kodi munthu ameneyu anali na udindo wanji ? Mu 535 B.C.E . , Koresi Wamkulu anagaŵanso madela amene anali kulamulila kukhala zigawo - zigawo . ( Luka 22 : 24 ) Ngakhale kuti io anali ndi maganizo olakwika cifukwa ca kupanda ungwilo , Yesu anadziŵa kuti otsatila akewo adzakhala Akristu ofikapo ndipo adzapanga mpingo wogwilizana . ( a ) Kodi Mfumu Solomo inalemba ciani pa nkhani ya kulimbikitsana ? Koma tingakwanitse kupewa kutengela maganizo na makhalidwe awo . Tingacite bwanji zimenezi ? Yehova anali atatsimikizila kuti adzapeleka ciweluzo kwa anthu acinyengo cifukwa ca zocita zawo zoipa . Patapita mawiki aŵili , mkulu wanga Bogdan , anafika kundende ina mumzinda wa Angarsk , pafupi ndi Tulun . Kodi tingatsatile bwanji malangizo a Paulo akuti ‘ tiziganizila ’ zofuna za ena ? Kodi nkhosa zingathandize bwanji abale a Kristu ? Mwacitsanzo , Yesu anafotokoza mafanizo ambili osavuta okamba za zinthu zimene anthu anali kudziŵa bwino . Anacita zimenezo n’colinga cakuti awafike pamtima . Komabe , kungakhale kulakwa kuganiza kuti Ophunzila Baibo anatengedwa ukapolo ndi Babulo Wamkulu monga cilango cawo ndi kuwawongolela . M’mapemphelo anu , mungaphatikizemo acinyamata , mabanja , atumiki a nthawi zonse , odwala , ndi aja amene ali ndi maudindo akuluakulu . Kodi tingaonetse bwanji kuti sitizengeleza pankhani ‘ yoleke kucita zosalungama ’ ? Abale ndi alongo ambili ocokela ku maiko akutali ( a zaka 19 mpaka 79 ) atumikila ku malo osoŵa ku Micronesia . ( Yobu 14 : 15 ) Yobu anali kudziŵa kuti ngakhale afe , Yehova adzalaka - laka kuukitsa mtumiki Wake wokhulupilika . Ngakhale kuti Adamu ndi Hava anapanduka , Yehova anafuna kuti mtundu wa anthu ukhale pa ubale ndi iye . Kanyumba kathu kanali kang’ono , koma tinali kukwanitsa kugonamo , kuphikilamo , ndi kuchapa zovala . Kucokela nthawi imeneyo , amayi ndiwo anatilela . ( b ) Kodi Petulo anakamba kuti tifunika kukhala na makhalidwe ati ? Ici ndi cosankha caumwini , ndipo sitiyenela kuneneza munthu amene wasankha kupezanso mnzake wina wa m’cikwati womuyenelela . — Aroma 7 : 2 , 3 ; 1 Akor . Atsogoleli acipembedzo a nkhondo acikatolika , amadalitsa magulu a nkhondo ndi zida zao pocita nkhondo ndi Akatolika a kumaiko ena . ( Agal . 6 : 4 ) Cifukwa copanda ungwilo , nthawi zina tingakhale ndi maganizo acinyengo m’mitima yathu . ( Aheb . Koma Mau a Mulungu asinthilatu umoyo wanga . M’malo motsatila maganizo a mkulu mmodzi , akulu onse omwe ndi “ mphatso za amuna ” zocokela kwa Mulungu amathandizana popanga zosankha zimene zimapindulitsa gulu la Yehova . — Aef . Popeza kuti Adamu sanamvele Mulungu , tonse ndife opanda ungwilo , tili ndi ucimo ndipo timafa . Iwo atulukilanso mmene magini a zamoyo amagwilila nchito . 25 : 46 . ( Aroma 16 : 17 , 18 ; Afil . Conco , Baibulo limanena kuti : “ Palibe munthu wolungama padziko lapansi amene amacita zabwino zokhazokha . ” — Mlaliki 7 : 20 . 97 : 10 ) Tisatengele anthu osaopa Mulungu , mwa kukamba kuti : “ Cabwino n’coipa ndipo coipa n’cabwino . ” Motelo , popita kumeneko usiku tinali kupita m’cipale cofewa . 33 : 22 ) Masiku ano , anthu ambili anzelu atsimikiza kuti mavuto amene ali pa dziko lapansi ni umboni wakuti anthu afunika thandizo la Mulungu . Khalani ozindikila : Musamangoona zimene ana anu amacita , koma muziganizilanso cifukwa cimene amacitila zimenezo . Ngati mumakhala kudela kumene kaŵilikaŵili kumacitika zinthu zosoŵetsa mtendele , mungafunse munthu kuti : “ Mungamve bwanji ngati lelo pa nyuzipepala pali nkhani yaikulu yakuti : ‘ Tsopano dziko lonse lili pamtendele , ndipo palibenso msokonezo . 5 : 12 ) Makalata ouzilidwa a Petulo akhala olimbikitsa kwa Akhristu kwa zaka zambili mpaka m’nthawi yathu ino . N’ciani cingacitike ngati makolo akonda coonadi ? M’madela ena , eninyumba amafuna kuti mukambitsilane zambili musanachule cifuno canu cowacezela . Mau a Ciperisiya akuti “ munda wochingidwa ” amatanthauzanso “ paradaiso . ” ( Mat . 5 : 23 , 24 ) Mwina mwakumbukila malangizo amenewa , amene Yesu anapeleka pa Ulaliki wake wa Paphili . Kodi timakonda kuŵelenga ndi kukhala oleza mtima pamene coonadi ca m’Baibulo cikumveketsedwa pang’onopang’ono ? Tsiku lina m’kilasi mwawo , anayamba kuphunzila nkhani yokhudza zipembedzo zosiyana - siyana . Luca anazindikila kuti buku limene anali kuseŵenzetsa pophunzila linali na mfundo zabodza ponena za Mboni za Yehova . Pa citsanzo ca banja la Yakobo , tikuphunzilapo kuti kukhala ndi mtima wokondela ndi watsankho m’banja kumasokoneza mgwilizano wa banja . Koma , ngati Satana anatenga Yesu mwacindunji ndi kupita naye ku kacisi weniweni , ena angafunse kuti : Muli na abale na alongo acikondi amene amakucilikizani . ( 1 Yohane 3 : 16 ) Kodi tingaonetse bwanji kuti timakonda abale athu ? Posacedwapa , mu January 2010 , civomezi coopsa kwambili cinacitika ku Haiti . Tiyeni tikambilane zozizwitsa zinai za Yesu . Mwa cisomo cake , Yehova anatipatsa mphatso ndi maluso osiyana - siyana . ( Ŵelengani Agalatiya 5 : 22 , 23 ; Akol . Kodi mwamuna angakwanilitse bwanji udindo wake mwacikondi ? Monga Atate wacikondi , Yehova anateteza ndi kudalitsa anthu 8 okhulupilikawo . ( Yakobo 3 : 2 ) Tiyelekezele kuti m’bale kapena mlongo winawake wakhumudwa cifukwa ca zimene munakamba kapena kucita . Mungagulitse , kupatsa ena , kapena kutaya zinthu zimene munaleka kuseŵenzetsa Kodi Adamu ndi Hava paciyambi anali ndi umoyo wotani ? Nanga pamenepa pabuka mafunso otani ? Monga mwa masiku onse , wofesa mbewu ‘ amagona usiku n’kudzuka kukacha . ’ M’mapikica ena , Yesu amaoneka ngati mngelo , kumutu kwake kuli nkhata yaciyelo , komanso wokonda kukhala yekha . Anapilila Zinthu Zopanda Cilungamo , ( Eliya ) , 2 / 1 Iwo amakonda kuuza uthenga wabwino anthu a m’midzi yakutali imene ili m’mbali mwa mitsinje imene imathila madzi mu Amazon Ca pa nthawiyi , makolo anga analandila mabuku kwa mmishonale wina wocokela ku England . Koma asanaone dziko lapansi likusintha kukhala paladaiso , io adzasangalala ndi cocitika cina pamodzi ndi Mfumu yao ndi olamulila anzake a kumwamba . Sitinganene motsimikiza . Koma cimene tikudziŵa n’cakuti Mariya ndi Yesu anamvela cifundo mwamuna ndi mkazi amene anali kukwatilana , ndipo anafuna kuwathandiza kuti asacite manyazi . Ndiyeno pambuyo pake , anapika jele zaka zina 10 . Komanso anatumizidwa ku dziko lina lakutali , kukakhala monga mkaidi kwa zaka 5 . Kodi sungawaonetse ulemu ? Timoteyo anali kukonda anthu na mtima wonse komanso anali kuika zinthu zauzimu patsogolo . 4 : 3 , 4 ) Nowa , Abulahamu , Isaki , Yakobo ndi Mose , onse anamanga maguwa a nsembe . ( Machitidwe 7 : 2 , 3 ) Pambuyo pakuti cisangalalo cawo catha , anayamba kuganizila za nchito imene Yehova anali atawapatsa . Mwacionekele , Akhiristu anapitiliza kucita zimenezo . Kodi Mulungu anamusiya ? Olo titakhala aluso bwanji , pali zinthu zina zimene sitingakwanitse kucita mwa mphamvu zathu zokha . ( Aefeso 4 : 22 - 24 ) Izi zitanthauza kuti tiyenela kupitilizabe kusintha ndi “ kuvala umunthu watsopano . ” 9 : 14 . Acinyamata ena makolo ao ndi a Mboni za Yehova , koma io safuna kutsatila mfundo za Yehova . Mwina mu mpingo mwanu mulinso abale na alongo a zitsanzo zabwino ngati amenewa . Mwina zinthu ngati zimenezi zikalibe kukucitikilamponi . Koma nkhawa zina zimene timakhala nazo mu umoyo zingakucititseni kukhala na mantha . Tikamaonetsa ena cikondi copanda dyela kapena ngati ena ationetsa cikondi cimeneci , timakhala na umoyo waphindu , komanso wodzala na cimwemwe . M’malo mwake , timamvela Yehova ndi kusintha ngati pafunika kutelo cifukwa cakuti timam’konda . 14 : 6 , 7 . Nanga anailemba liti ? Kodi inuyo mumayamikila mphatso imene Yehova wakupatsani omwe ndi akulu ? [ Mau apansi ] Amakondwelanso akaona mgwilizano umene ulipo pakati pa odzozedwa ndi a nkhosa zina , amene amamvetsela mokhulupilika ndi kutsatila M’busa wao , Yesu . Mafunsowo anandicititsa kuyamba kuganizila kwambili za utumiki wanga . ” Kwa zaka zambili , zofalitsa zathu zakhala zikufotokoza kuti Gogi wa Magogi ndi dzina limene Satana Mdyelekezi anapatsidwa kucokela pamene anacotsedwa kumwamba . Iye adzakupatsani mtendele wamaganizo kuti mulimbane ndi vuto lililonse . — Sal . Monga taonela , kudzikonda pa mlingo woyenelela kulibe vuto , komanso ndalama pazokha zilibe vuto . Cotelo , Timoteyo anafunika kukhala wotsimikiza kuti coonadi cimapezeka m’Malemba . Yehova Mulungu adzaika “ maganizo ake ” m’mitima ya “ nyanga 10 ” za ‘ cilombo cofiila kwambili . ’ Kodi tikambilana zinthu zofunika ziti ? 16 : 26 - 40 ) Zinthu zinasinthadi mofulumila kwambili ! ( Onani pikica pamwambapa . ) ( b ) N’cifukwa ciani kukumbukila zifukwa zimene timagwilila nchito yolalikila n’kofunika ? Ciphunzitso cakuti mzimu sukufa n’cimodzi mwa “ ziphunzitso za ziŵanda . ” Kuceza nawo mwanjila imeneyo kunanilimbikitsa ngako . M’nkhani ino ndi yotsatila , tidzakambilana mfundo zamtengo wapatali za m’buku la Levitiko , zimene zidzatithandiza kukhala oyela polambila Mulungu . Ngakhale kuti nthawi zambili iwo anali kukumana m’nyumba za Akhristu anzawo kuti alambile Mulungu , sanaleke kuimba nyimbo zotamanda Yehova . Popeza iye ndiye anatilenga , tiyenela kumuyamikila , kumulemekeza , ndi kumutamanda . Mboni za Yehova zimasangalalabe ndi ciyembekezo cawo ngakhale pamene zikuzunzidwa moopsa . Limodzi mwa mavuto amene Yesu anakamba kuti otsatila ake afunika kuwapilila ni citsutso ca m’banja . ( Mat . 5 : 11 ; 2 Pet . Iye ndi Mfumu komanso Mkulu wa Ansembe wacifundo kwambili . Anatsutsa atsogoleli acipembedzo molimba mtima cifukwa cosoceletsa anthu ndi ziphunzitso zabodza . Komabe zinthu zinali kudzasintha mwadzidzidzi . Akulu - akulu a bomawo atauzidwa kuti Paulo na Sila ni nzika za Roma , anazindikila kuti awalakwila kwambili . 24 : 14 . Kodi Mudzayembekezela Moleza Mtima ? Ambili amene amapanga cosankha cimeneci ndi acinyamata , ndipo ena amakhala kuti sanakwanitse zaka 13 . Mwacitsanzo , mfumu ya Yuda , Uziya , anali wokhulupilika kwa zaka zambili . Pakati pa acinyamatawo panali mtsikana wina dzina lake Laurie , amene anadzakhala mkazi wanga . Wamasalimo Davide , amene anali mwamuna wamphamvu ndi wolimba mtima , anati : “ Ngati mwakwiya , musacimwe . 11 : 9 ) Aliyense amene adzakhala mmenemo azikaphunzitsiwa na Mulungu . Kumene tinali kukhala nyengo inali yabwino , ndipo umoyo wathu unali wabwino . Kodi n’ciani cingakuthandizeni ? Kodi muli ndi wacibale amene amakutsutsani ? Pa lembalo timaŵelenga kuti : “ Nditayang’ana , ndinaona hachi yoyela . Wokwelapo wake ananyamula uta . Mafanizo abwino angathandizenso mwana kukhulupilila kuti Baibulo n’loona . Tizipeleka mapemphelo oyamikila pa zabwino zimene amaticitila . ( Miy . 3 : 5 , 6 ) Conco , tiyeni nthawi zonse tizidalila Yehova amene amatipatsa zinthu zabwino ndi kutiteteza kuposa wina aliyense . M’malo mothandiza anthu wamba kumvetsetsa Baibo , Baibo imeneyi inacititsa kuti anthu azilephela kuimvetsetsa , cifukwa m’kupita kwa nthawi anthu sanali kudziŵa Cilatini olo pang’ono . Ndiye cifukwa cake Baibo imati : “ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” 5 , 6 . ( a ) Kodi Mikayeli ndani ? Cakudya cimakhalako cambili koma zimafunika kuyenda kukacisakila na kucipeza . Mofananamo , anthu a Yehova masiku ano pofuna kukhala a aukhondo , amapewa kugwilizana ndi anthu a mumpingo amene amanyalanyaza malamulo a Yehova . Popeza Baibo sikamba kuti anthu ali ndi cinacake m’thupi mwawo cimene ena amati mzimu umene sukufa , n’cifukwa ciani machechi ambili amaphunzitsa zimenezi ? ( Yohane 1 : 18 ) Popeza Yesu ndi colengedwa coyamba ca Mulungu ndipo iye ndi Mwana wobadwa yekha , anakhala maso athu oonela kumwamba . Tikatelo , ndiye kuti mfundo zatsopano za coonadi zidzakhazikika mumtima mwathu . Satana Mdyelekezi anaseŵenzetsa njoka kunyenga Hava kuti asamvele Atate wake , Yehova . 3 Kodi Mudzayembekezela Moleza Mtima ? Tiyenela kukumbukila bwanji imfa ya Yesu ? ( Aef . 2 : 6 ) Iwo anapatsidwa mwai umenewu cifukwa cakuti ‘ anaikidwa cidindo ca mzimu woyela wolonjezedwawo , umene ndi cikole ca coloŵa cao cam’tsogolo , ’ kutanthauza ‘ ciyembekezo codzalandila zimene awasungila kumwamba . ’ — Aef . Mwacitsanzo , Innocent wa ku Nigeria wa zaka 72 amakonda kuceza ndi anzake . Ndiponso Mulungu amadana ndi “ munthu wokhetsa magazi ndi wacinyengo . ” Masiku ano , tili na mipingo 83 na tumagulu 25 tumene tumacita misonkhano m’Cichainizi , Cizungu , Cikigizi , Cirasha , Cinenelo ca Manja ca ku Russia , Citeki , Ciwiga , na Ciuzibeki . Timafunika kusonkhela nkhuni pa moto kuti uyake kwambili . Kodi nkhani ya Loti ndi ana ake aakazi ikutiphunzitsa ciani pankhani ya kukhala ogwilizana kwambili ? Pali ubwino waukulu ngati ticitila anthu amene timalalikila zinthu zimene tingafuna kuti io aticitile . * Mabanja ambili asiya nyumba zao zokongola , nchito zabwino , ngakhale ziweto zao , kuti atumikile Yehova mokwanila . ( Gen . 12 : 1 - 3 , 7 ) Abulahamu mu ukalamba wake anapempha kuti : “ Yehova Ambuye Wamkulu Koposa , mudzandipatsa ciani ine ? Taonani ndilibe mwana . . . Ndi umboni wotani umene ulipo wakuti Yesu anaukitsidwadi ndipo ali moyo ? Mosasamala kanthu kuti Yehova analola zinthu zopanda cilungamo kucitika , pamapeto pake zinathandiza pa “ kuteteza uthenga wabwino ndi kukhazikitsa mwalamulo nchito ya uthenga wabwino . ” ( Afil . Mwacitsanzo , Mose , mtsogoleli woyamba wa mtundu wa Isiraeli , “ anayamba kufotokoza ” zinthu zolembedwa . — Deuteronomo 1 : 5 . Monga zinalili m’nthawi ya Zekariya , Yehova wa makamu akali kuseŵenzetsa angelo poteteza na kulimbikitsa anthu ake . ( Mal . 3 : 6 ; Aheb . 15 : 51 , 52 . Anzanga ambili akale anafa ndipo ena ali m’ndende , koma ine ndili ndi moyo wokhutilitsa ndi tsogolo labwino kwambili limene ndi kuliyembekezela . Ndinali kukondwela kulemba sigineca yanga pa zinthu za anthu , kulandila maluŵa , ndi kuona anthu akundicemelela . Mwina anthu ambili m’madela amenewo alibe luso logwilila nchitoyo kapena alibe zipangizo zogwilitsila nchito . Musawaone ngati osafunika , ndipo musawapewe poona kuti ni ocititsa manyazi . ” Zipembedzo zonama zimatenga mbali m’ndale , ndipo zimenezi zimagaŵanitsa anthu . ( Miy . 22 : 3 ) Ndipo ngati mwayesedwa kuti mucite ciwelewele muzikana mwamsanga . — Gen . Izi ziyenela kuti zinamulimbikitsa . M’bale Paul amene tachula uja , amene anatenga udindo wa m’bale Peter woyang’anila dipatimenti pa Beteli , anati : “ N’nali kufunsila uphungu kwa m’bale Peter , ndipo n’nalimbikitsanso ena mu dipatimenti yathu kuti azicita cimodzi - modzi . ” Iye anali kuwamvela ndi kukhala wokhulupilika kwa io osati cifukwa cakuti anali kufunika kucita zimenezi , koma cifukwa cowakonda . 27 Mungapambane Bwanji Nkhondo Yoteteza Maganizo Anu ? Mtumwi Paulo anapeleka cenjezo liti kwa anthu a Mulungu m’nthawi ya atumwi ? 13 : 1 ; Mac . 13 : 21 . Afunika kukamba zabwino ponena za makolowo , osati kucita ngati afuna kuwalanda udindo . Kodi mungacite ciani ? Munthu amakhala ndi cikhulupililo mumtima mwake kuti akhale wolungama , koma ndi pakamwa pake amalengeza poyela cikhulupililo cake kuti apulumuke . ” — Aroma 10 : 9 , 10 ; 2 Akor . Iwo analibe nthawi yoceza ndi kusonyezana cikondi monga mwamuna ndi mkazi . ( Nyimbo 1 : 2 ; 1 Akor . 8 : 24 . Baibo imatilangiza kuti ngati tili na nkhawa iliyonse , tiyenela ‘ kum’tulila Yehova . ’ Ezekieli anaona masomphenya a cigwa cimene cinali ndi mafupa okhaokha . ( Akolose 3 : 12 - 14 ) Ndife oyamikila kuti pakati pathu , tili ndi cikondi cimene “ cimagwilizanitsa anthu mwamphamvu kwambili kuposa cinthu cina ciliconse , ” mosasamala kanthu za kumene tinacokela . 13 : 4 , 5 ) Mukasiyana maganizo , kambilanani mwamsanga kuti vutolo lithe . N’cifukwa ciani lemba la Salimo 45 ndi locititsa cidwi kwa ife ? Mofanana na mbalame zina zokuka - kuka , adokowe ‘ amadziŵa nyengo yobwelela kumene anacokela . ’ — Yeremiya 8 : 7 . Aliyense m’banja anayembekezela kuti ndidzatumiza mwana wanga kunyumba kuti makolo anga akamulele mpaka titapeza ndalama zambili . ” Nanga tingacite ciani kuti ‘ tilole kupilila kumaliza kugwila nchito yake ’ ? — Yakobo 1 : 4 . ( Aroma 3 : 1 , 2 ) Komabe , pofika m’zaka za m’ma 200 B.C.E , Ayuda ambili sanali kumvetsetsa Ciheberi . Akaona mau amenewa mu Uthenga Wabwino wa Mateyu , ambili amakamba kuti : “ Ndakhala ndikufunitsitsa kuŵelenga Baibulo ngakhale kamodzi kokha . ” Panthawi ina ali ndi zaka pafupifupi 17 , atate ake , a Yakobo , anam’tuma kuyenda ulendo wa makilomita ambili kucoka kunyumba kwao . ( Akol . 3 : 15 ) Tonse timakonda Mulungu mmodzi , timalalikila uthenga wofanana , ndipo mavuto ambili amene timakumana nawo ni olingana . “ Mukhulupilileni nthawi zonse , anthu inu . ” — SAL . Koma cifukwa cakuti Mlengi wathu amadziŵa zambili , iye amaona ngati zimene tipempha n’zofunikiladi . ( Salimo 25 : 4 ) Nthawi zambili , Yehova amayankha mapemphelo athu kudzela m’Baibulo . Nthawi zambili , ngati tikamba za abale ndi alongo amenewa timanena kuti akutumikila kumalo osoŵa . ( Miyambo 17 : 17 ) Kodi zingakhale kuti ndi Yehova anasonkhezela mnzathuyo ? ( Mateyu 24 : 20 , 21 ; Aheberi 12 : 4 ) Akristuwo anafunika kupilila ndi kukhala ndi cikhulupililo colimba kuti amvele malangizo a Yesu akuti athawe m’madela ao . Akanapanda kutelo , akanaphedwa . Anna anati : “ Tsiku lina , n’nalalikila mtsikana wina wa pa univesiti ku maketi na kupangana naye kuti tidzakumanenso . ( Genesis 1 : 28 ; Salimo 37 : 29 ) Koma Yehova amasankha anthu ena kuti adzakhale mafumu ndi ansembe kumwamba . Kodi mkate ndi vinyo za pa Cikumbutso tiyenela kuziona motani ? Amatithandiza kuti tizicita zabwino . 12 : 13 , 14 . Patapita zaka zambili , Yehosafati , mfumu ya Yuda , inalamula kuti : “ Samalani zocita zanu cifukwa simukuweluzila munthu koma mukuweluzila Yehova , ndipo iye ali nanu pa nchito yoweluzayi . 27 Muzicitila Cifundo Anthu , “ Kaya Akhale a Mtundu Wotani ” 2 : 17 ) Umenewu ndi mwai waukulu kwambili . Ngati Mulungu anapanga cilengedwe conse , iye sangalephele kutipatsa Baibulo ndi kuiteteza . Iye anati : “ Pamene ndinacotsedwa ndinazindikila kuipa kwa khalidwe langa . ( Ŵelengani Salimo 110 : 3 ; Mac . 6 : 1 - 3 ) Mtumwi Paulo anatenga Timoteyo pa ulendo wa umishonale cifukwa “ abale . . . anamucitila umboni wabwino . ” — Mac . 16 : 1 - 5 . Mungacite zimenezi mwa kupeza nthawi yoŵelenga Mau ake ndi kusinkhasinkha pa zimene mukuŵelenga . ( Yesaya 40 : 31 ) Ciwombankhanga cimaseŵenzetsa mphepo yothuma kuti ciuluke m’mwamba kwambili . ( b ) Kodi kulalikila mwaluso kumangodalila pa kukhala aphunzitsi abwino ? Nakhala na mwayi wotumikila monga mpainiya wa nthawi zonse kwa zaka 23 tsopano . ( Yobu 14 : 1 ) Kodi tingawasamalile bwanji ? Meriba uyu ni wina osati uja wa kufupi na ku Refidimu . Nchito yofalitsa coonadi ca Ufumu ikupitilizabe , ndipo siidalila munthu mmodzi m’gulu la Yehova . Koma munthu woika maganizo pa zinthu za mzimu ni amene moyo wake wonse umakhala pa kucita zinthu zokhudzana ndi kulambila Mulungu , ndipo amayesetsa kugwilizanitsa maganizo ake ndi a Mulungu . Pamene tiŵelenga Buku Lapacaka , timasangalala kumva zotsatilapo za nchito yolalikila padziko lonse lapansi . Pali Ciyembekezo Cotani Ponena za Makolo Anga Akale ? Cifukwa cakuti Mulungu wathu wacikondi amacitila atumiki ake okhulupilika zinthu zabwino nthawi zonse . ( Yobu 4 : 18 , 19 ) Mfundo imeneyi iyenela kutithandiza kudziŵa kuti ndife ofunika mumpingo , ndi kuti tili mbali ya gulu la Mulungu la padziko lonse . Ŵelengani Mateyu 6 : 25 . Yelekezelani kuti mukumuona akuthawa kuti abisale kwa adani ake . Akucita mantha ndi anthu amene akwiya cifukwa cowauza uthenga wocokela kwa Mulungu . Nafenso tsiku lina tingapezeke m’mkhalidwe wa conco . Maurizio nayenso ananithandiza pa nthawi imene ine n’nali kufunikila thandizo . Hava nayenso anakonda kwambili mwamuna wake . Ndipo mpake kuti anatelo cifukwa Yehova analenga Hava kucoka kwa Adamu . Koma pambuyo pofufuza moonjezeleka , tazindikila kuti anthu a Mulungu anakhala akapolo kwa zaka zambili cisanafike caka ca 1918 . Iye anati : “ Colinga canga cinali kufuna kukhomeleza coonadi m’mitima mwa ana anga mwa mau ndi zocita , osati cabe kunena kuti ndimakonda Yehova . ” ( 1 Yoh . 17 , 18 . ( a ) Ndi zida zina ziti zimene Satana amagwilitsila nchito ? Pambuyo pa ubatizo wake , mwamsanga Yesu anayamba kulengeza “ uthenga wabwino wa ufumu wa Mulungu ” kulikonse . Cinanso , muyenela kudziŵitsa akulu kuti ndinu wokonzeka kuthandiza pa nchito iliyonse , kaya ni yoyeletsa pa Nyumba ya Ufumu , kukambako nkhani za volontiya pa misonkhano , kapena kutengako winawake m’motoka yanu popita ku misonkhano . Ayi ndithu , sanamulandile . Koma upainiya unaniphunzitsa kukamba ndi anthu a mitundu yonse . 15 : 22 ) Mwamuna wacikondi sakakamiza mkazi wake kuti azimulemekeza , koma amayesetsa kucita zinthu zimene zingacititse mkaziyo kuyamba kum’lemekeza . 115 : 16 . Ndinakhudzika mtima kwambili cakuti misozi inagwa m’maso mwanga . ( b ) Kodi tiphunzilapo ciani pa zimene zinacitikila angelo ena ambili ? ( 2 Timoteyo 3 : 16 , 17 ) Tsopano , io ‘ akuyenda m’njila [ za Mulungu ] ’ ndipo iye amawakonda ndi kuwateteza . Pa Pentekosite mu 33 C.E . , ophunzila a Yesu odzozedwa atsopano anadziŵitsa anthu “ zinthu zazikulu za Mulungu , ” ndipo ambili amene anamvetsela anacitapo kanthu . Kuti mudziŵe cifukwa cimene Mulungu wololela zinthu zoipa kupitilizabe , onani nkhani 11 , m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni - ceni lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . 24 : 15 ) Yehova afuna kuti anthu akhale ndi moyo , osati kufa . “ Tate wanu amadziŵa zimene mukufuna . ” — MAT . Ndi uphungu uti wa m’Malemba umene ungatithandize kupitilizabe kukonda anzathu ? Kusatengako mbali m’nkhondo kwa Mboni za Yehova kwakhudza bwanji owaona ? ( Mac . 1 : 9 , 10 ) Kwa zaka ziŵili , Yesu anali kuwaphunzitsa , kuwalimbikitsa , ndi kuwatsogolela . ( Ower . 6 : 15 ) Koma pamene analandila udindowo kwa Yehova , Gidiyoni anayesetsa kuumvetsa udindo wake na kuusamalila bwino lomwe . Citsanzo cake cingatithandize kukhalabe ndi maganizo oyenela ngakhale kuti sitingathe kucita zambili . Ndiyeno , wiki yokonkhapo , ine n’nacezetsa mpingo wina ndipo wadelayo anali kuniyang’anila . “ Inunso khalani oyela m’makhalidwe anu onse . ” — 1 PET . Mofananamo , Yehova amatithandiza kukhalabe olimba m’cikhulupililo . Yesu anauza otsatila ake kuti simufunika kucita “ kukonzekela zoti mukayankhe podziteteza , cifukwa ine ndidzakuuzani mau oti munene ndi kukupatsani nzelu , zimene otsutsa anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa . ” — Luka 21 : 14 , 15 ; 2 Tim . 27 ‘ Zimenezo Uziphunzitse kwa Amuna Okhulupilika ’ Kodi kugwilitsila nchito nthawi yathu kukonzekela kudzakhala m’dziko latsopano la Mulungu , kutanthauza kuti tiyenela kunyalanyaza zinthu zina zimene zingatithandize kukhala okhutila masiku ano ? Nkhani ziŵilizi zifotokoza mmene makolo angatengele citsanzo ca Yesu ca mmene anali kuphunzitsila ophunzila ake . Zifotokozanso mmene angatengele citsanzo cake ca kudzicepetsa , cikondi , ndi kuzindikila . Pa anthu onse amene anakhalapo pa dziko , Yesu ndiye citsanzo cabwino ngako ca munthu wauzimu . ZAKA zingapo zapita , mlongo wina anali kukambitsilana Baibulo ndi mwamuna wake wosakhulupilila . Cina , tiyenela kumvela malangizo awo ocokela m’Malemba . Patapita zaka 300 Baibo itatha kulembedwa , katswili wina wa zacipembedzo dzina lake Jerome anatulutsa Baibo ya m’Cilatini , imene m’kupita kwa nthawi , inadzachedwa Latin Vulgate . ( Mateyu 4 : 1 - 4 ) Conco , Mdyelekezi si cinthu congoyelekezela kapena maganizo oipa a munthu . Kodi dzina lakuti Yehova lingatanthauzenji ? Tikapanikizika kapena ena akatiputa , zimakhala zovuta kukhalabe wofatsa . Zinthu zoipa komanso makhalidwe oipa amene akuculukila - culukila masiku ano , ni umboni wakuti iwo ni okwiya maningi . — Chivumbulutso 12 : 9 - 12 . Kuti tikhale otetezeka , timapatsidwa zikumbutso kudzela m’gulu la Yehova ndi m’zofalitsa zathu . Koma anali wacibululu wapatali wa Abulahamu , Isaki na Yakobo , anthu amene anali kudziŵa coonadi ponena za Yehova na colinga cake kwa anthu . Iwo anati : “ Tiyenela kukumana ndi masautso ambili kuti tikaloŵe mu ufumu wa Mulungu . ” — Machitidwe 14 : 20 - 22 . Kodi Yehova waonetsa bwanji kuti ni Mulungu amene amapeleka cilimbikitso ? Ngati ndinu kholo ndipo munasamukila m’dziko lina , kodi mungawaphunzitse bwanji ana anu kukonda zinthu zauzimu ndi kupitiliza “ kuyenda m’coonadi ” ? ( 3 Yoh . * Nanga zipatso zimene otsatila a Khristu afunika kubala n’ciani ? Mwana amene anapempha atate wake kuti amupatse colowa cake kenako n’kuononga cumaco akuimila anthu amene anasocela ndi kucoka mumpingo . Izi n’zimene Baibulo limanena kuti : “ Cilakolako cikatenga pakati , cimabala chimo . ” — Ŵelengani Yakobo 1 : 14 , 15 . Kumeneko , tinali kulalikila mosamala m’matauni apafupi , kumene anthu ocokela kumadela osiyana - siyana a dzikolo anali kubwela kudzasangalala . Cikondi cimabweletsa cimwemwe cifukwa . . . Kodi cikondi ca Mulungu cimatipatsa cidalilo cotani ? Pambuyo pake , Tessie anabatizika ndi kukhala mpainiya wa nthawi zonse ngakhale kuti anali ndi ana aang’ono . Anali paubale wabwino ndi Mlengi wao monga ana ake . ( Gen . Atumiki a Yehova akale anapeleka citsanzo cabwino pankhani yolemekeza ndi kumvela olamulila . Baibulo imati : “ Anayamba kumudelela cifukwa anali mnyamata wamaonekedwe ofiilila , ndiponso wokongola . ” Ngati timakonda Yehova na kum’tumikila cifukwa cakuti ni wabwino ndipo ndiye woyenela kulamulila cilengedwe conse , sitidzakopeka ngakhale pang’ono na bodza la Satana . Ganizilani zimene zinacititsa kuti iye agonjetsedwe ndi kuphedwa . Nthawi zina , kucita izi kungakhale kovuta . Kodi pali zinthu zina zimene tingacite zogwilizana ndi pempho lacinai lokhudza cakudya cathu calelo ? — Ŵelengani Mateyu 6 : 11 - 13 . Baibulo limatilimbikitsa kuti , “ khalani maso kuti musanyalanyaze kupemphela . ” ( Aheberi 10 : 5 ; Mateyu 3 : 13 - 17 ) Kodi thupi limenelo linali kuoneka bwanji ? “ Kuopela kuti Satana angapitilize kumakuyesani mukalephela kudzigwila . ” Izi zitanthauza kuti tiyenela kulambila Yehova yekha cabe , ndi kumumvela na mtima wathu wonse . Sicopepuka kukamba kuti “ Pepani , ” koma zimenezi ndi zimene zimathandiza kuthetsa mikangano . Angatenge bola ( mpila ) kapena mwala ndi kuonetsa kuti cinthu ciliconse colema sicingakhazikike m’malele . Mbuyeyo analanda kapolo woipa talente yake ndi kupatsa kapolo woyamba . Panopa tikudziŵa kuti mafanizo amenewa amanena za Ufumu wa Mulungu , umene wathandiza anthu ambili kukana dziko loipali ndi kukhala ophunzila a Kristu . Timapindula bwanji ngati tikambilana za ciyembekezo cathu ? Mwacitsanzo , iye anapanga dzuŵa , limene ndi lamphamvu kwambili . Atate Ake a Yosefe , Na . Iye adzacita zimenezi mtsogolo pa nthawi ya cisautso cacikulu . Cifukwa cakuti ngati nthawi zonse tikumbukila zifukwa zake tiyenela kupitiliza kulalikila , timalimbikitsidwa kupilila pocitila “ umboni ku mitundu yonse . ” ( Mat . ( Chiv . 4 : 11 ) Ife tonse tidzapindula kwambili ngati timapenda zocita zathu ndi kucotsa cinyengo ciliconse m’mitima yathu . Popeza zocitika zimasiyana - siyana , pangakhalenso mfundo zina zimene akulu angapende . Nditabwelela ku Austria , ndinayamba kutumikila ku dela lina kumene ndinakumana ndi Tove Merete , mlongo wokongola , amene anali mbeta . Anali okoma mtima ndi odekha , ndipo izi zinanicititsa cidwi kwambili . Kodi Yehova afuna kuti mukhale na zolinga zotani ? Kodi Petulo anapindula bwanji cifukwa cokhululukidwa na Yehova ? Ngati timaona utumiki wathu monga cuma , tidzatsatila citsanzo ca mtumwi Paulo mwa kupitilizabe kulalikila olo tikumane na cizunzo . Kholo lakale Yakobo , anacilimika cifukwa cokonda Yehova na zinthu zauzimu . Anakhulupililanso kwambili lonjezo la Yehova lakuti adzadalitsa mbeu yake . Nkhani zambili zimakhala zoona , zothandiza , ndiponso zabwino . Mu 1958 , n’nakwatila Lene , mlongo wa ku Denmark amene anali kukhala mu London . ( Genesis 24 : 50 - 54 ) Kodi zimenezi zitanthauza kuti Rabeka analibe ufulu wokambapo pa nkhaniyi ? A Zimba : Zikomo . Koma m’buku la Mau ake , Yehova amapeleka mayankho pa mafunso amene avutitsa anthu maganizo kulikonse . Papa anaonjezela kuti nchito yolalikila siyenela kugwilidwa ndi anthu ocepa cabe amene anaphunzitsidwa koma ndi mamembala onse a cipembedzo . Mu 1933 , anadutsa cipululu ca mcenga cochedwa Simpson kuti akalalikile m’tawuni yochedwa Alice Springs , m’kati mweni - mweni mwa dzikolo . Yesu anati : “ Aliyense wocita cifunilo ca Mulungu , ameneyo ndiye m’bale wanga , mlongo wanga ndi mai anga . ” — Maliko 3 : 35 . Iye anadziŵa kuti zocita za anthu zidzaonetsa kuti io alephela kudzilamulila . Tsopano tamudziŵa mkwati , koma kodi mkwatibwi wake ndani ? Cinthu cimene abale ake a Yosefe analephela kumulanda cinali cikhulupililo . Ngakhale kuti nesiyo anali wamkuluko kuposa ine , anali ndi nkhawa kwambili . Conco , ndi bwino kupewa kupatuka kwa Mulungu , mwa kucitapo kanthu mwamsanga kuti tipewe kucita chimo . 5 : 10 - 12 . Koma ngati tiyesetsa kukulitsa khalidwe la cifundo , zimakhala ngati tikuwonjezela nkhuni pa moto . Cangu cathu mu ulaliki cimapitiliza kuyaka ngati moto . — 1 Ates . 13 : 15 . 1 : 8 , 9 . Kodi mukudziŵa tanthauzo la zocitika zimenezi ? “ N’cifukwa Ciani Ndimaopa Kuuza Anzanga a Kusukulu Zimene Ndimakhulupilila ? ” — mutu 17 Conco , tadziŵa zimene zimacitika tikamwalila ndipo sitifunikilanso kucita mantha . Yehova amatigwilitsila nchito monga anchito anzake , mosasamala kanthu ndi zofooka zathu ndi kupanda ungwilo kwathu . Kodi mungacite bwanji ngati mwaona kuti mwacitilidwa zinthu zopanda cilungamo mumpingo kapena ngati Mkhristu mnzanu wakulakwilani ? A Zimba : Inde . 34 : 6 ; Yobu 2 : 2 - 6 ) Motani ? Yehova walola kuti papite nthawi yaitali cifukwa safuna kuti aliyense adzawonongedwe , koma “ amafuna kuti anthu onse alape . ” — 2 Pet . Koma nthawi zina kucita zinthu mwamsanga kuti mudziteteze kumaonongelatu zinthu . Kuti mupulumuke cisautso cimene cikubwela , mufunika kucitapo kanthu mwamsanga . ( 2 Akor . 5 : 18 , 19 ) Conco , mwa kulalikila uthenga wabwino ndi mtima wonse , timaonetsa kuti timakonda anzathu m’njila yofunika kwambili . M’magazini athu mumakhalanso nkhani zabwino zofuna kuseŵenzetsa luso la kulingalila . Cimene cionetsa kuti anali munthu wauzimu ni mau abwino acitamando amene iye anakamba pamene anakacezela abululu ake , Zakariya na Elizabeti . Pamene a Mboni anandipempha kuphunzila Baibulo ndinavomela . 24 : 30 , 42 , 44 ) Motelo , pamene Yesu anakamba kuti “ mbuye wa akapolowo anabwela ndi kuŵelengelana nao ndalama , ” iye anali kutanthauza nthawi imene iye adzabwela kuweluza anthu ndi kuononga dziko la Satana . Koma kuganiza conco kungakhale kosemphana ndi lamulo la Mulungu limene limati : “ Usabwezele coipa kapena kusungila cakukhosi anthu a mtundu wako . ” ( 3 Yoh . 7 ) Popeza kuti abalewa anali mbali ya mpingo wacikhristu , anafunika kulandilidwa bwino . ( Mateyu 14 : 14 ) Yesu nayenso ali ndi mphamvu zolamulila cilengedwe . M’Cigiriki , kalata imene mtumwi Yohane analembela Gayo ili na mau 219 cabe , ndipo kalata imeneyi ndiyo buku lalifupi kwambili m’Baibo . Posakhalitsa , n’naphunzila mfundo ina m’Baibo imene inasintha umoyo wanga . N’ciani cingatithandize kusankha zosangulutsa zoyenela ? 12 : 17 ) Tinapanga cosankha cotumikila Yehova ndi kusunga malamulo ake . Anthu ochulidwa m’Baibo monga Abisalomo , Uziya , ndi Nebukadinezara , anakhala odzikuza cifukwa cogonja ku “ nchito za thupi . ” Ndipo Yehova anawatsitsa mocititsa manyazi . — 2 Sam . Caciŵili , Ezekieli anaona anthu akufa akukhala ndi moyo mwapang’onopang’ono osati mwadzidzidzi . Yesu anali wozindikila ndipo anali kudziŵa mmene angathandizile ophunzila ake . Ndi mwai wamtengo wapatali kulandila zinthu zambili kucokela kwa Mulungu . ( a ) Kodi Akristu odzozedwa amakono ananenelatu za caka citi capadela ? Nawonso atsogoleli aciyuda anali kuona otsatila a Yesu kukhala otsika . Ndipo pamene abale ake anabwela ku Iguputo ndi kugwilizananso ndi Yosefe , Farao anawalandila ndi kuwalola kukhala m’dziko la Iguputo kuti azisangalala ndi “ zabwino za dziko lonse la Iguputo . ” — Gen . Ngakhale ndi conco , io alephela kugonjetsa imfa . Iye anadziŵa kuti Mulungu afuna kuti ‘ alengeze uthenga wabwino kwa osauka ’ ndi ‘ kulalikila . . . zoti akhungu ayambe kuona . ’ Fotokozani . Ndimamva cisoni ndikaganizila zinthu zambili zimene zinaonongeka cifukwa ca nkhondo yaciŵili ya padziko lonse . Kodi uli na malile ? Mwambo wokumbukila imfa ya Yesu unali kupeleka mwai wosinkhasinkha mwakuya pa zimene zinacitika . ( b ) Kodi Akristu anapindula bwanji ndi lamulo la Aroma ? ( a ) Ndi phunzilo lotani limene tikuphunzilapo pa fanizo la kanjele ka mpilu ? Ndipo , tidzaphunzilanso malo a akazi Acikristu m’kakonzedwe ka Mulungu masiku ano . M’malo mwake , anawatsekela m’malo a “ mdima [ wauzimu ] wandiweyani ” ochedwa Tatalasi . Ngati mai sanakwanitse kupeleka nkhosa , iye anali kuloledwa kupeleka ana a nkhunda aŵili kapena njiŵa ziŵili . M’mizinda imeneyi nthawi zambili munali kumveka phokoso la “ kupela kwa mphelo . ” ( Miy . 2 : 3 - 6 ) Uziseŵenzetsa zida zofufuzila zimene zilipo m’cinenelo canu , monga DVD ya Watchtower Library , LAIBULALE YA PA INTANETI , komanso Watch Tower Publications Index , kapena Buku Lofufuzila Nkhani la Mboni za Yehova . N’nayesetsa kupewa kulila pamaso pa amayi , koma nikakhala kwanekha n’nali kulila kwambili . M’malomwake , anayamba utumiki wa nthawi zonse . ( 1 Akor . 14 : 9 ) Tinali kukaikila kuti gulu la Mulungu lingatulutse zofalitsa m’Cituvalu cimene cinali kukambidwa ndi anthu osakwana 15,000 . Kodi tingacite ciani kuti tikhale ogwilizana m’banja ? Nthawi zina , mlongoyo anali kumva kuti m’nyumbamo munali munthu koma sanali kuyankha . Ifotokozanso cifukwa cake tifunika kukhulupilila kuti Yehova adzatipulumutsa pa cisautso cacikulu . Mwacitsanzo , Yehova wayembekezela moleza mtima kwa zaka zambili - mbili kuti nkhani zimene zinabuka m’munda wa Edeni zithetsedwe moyenelela . Kodi tingatengele bwanji citsanzo ca Yesu pokamba ndi anthu ? Koma iye anandiuza kuti sindiyenela kuwaŵelenga cifukwa Mboni za Yehova sizimam’khulupilila Yesu . Amuna ayenela kucitila akazi awo “ mowadziŵa bwino . ” ( 1 Pet . Kodi iye anacita mantha ataganizila za cizunzo ? Kuyelekezela mwanjila imeneyi n’koyenela . Baibulo limati : “ Ndiyeno Yehova Mulungu anapatsa munthuyo lamulo lakuti : ‘ Zipatso za mtengo uliwonse wa m’mundamu uzidya ndithu . Cifukwa ca zimenezi , n’natengelapo mwayi woleka sukulu n’kuyamba kugwilizana ndi anzanga ena . Kodi pemphelo ndi kusinkhasinkha zingatithandize bwanji kukhalabe oyamikila ? Ndiyamikila kwambili kuti Yehova wandithandiza kuyamba utumiki wa nthawi zonse umenewu . Coonadi ‘ Sicibweletsa Mtendele Koma Lupanga , ’ Oct . Mboni za Yehova zimadziŵika kuti ndi otsatila a Kristu oona cifukwa cakuti amakondana ndi kugwilizana , ndipo Mulungu akuwagwilitsila nchito kulalikila uthenga wabwino wa Ufumu padziko lonse “ Sindikupeza munthu woti ndingakwatilane naye mumpingo , ndipo ndikuopa kuti ndingakalambe ndili mbeta . ” Kodi mumauona bwanji utumiki wanthawi zonse ? Pambuyo pake , Rabeka , Debora , amene anali mlezi wake , ndi adzakazi ena anapitila pamodzi ndi Eliezere ndi anyamata ake . Mosiyana ndi zimenezi , munthu wocita mau ‘ amayang’anitsitsa m’lamulo langwilo ’ ndipo “ amalimbikila kutelo . ” Zimene anakamba Steve na Ulf , zitikumbutsa mau a pa Salimo 19 : 7 , 8 , amene amati : “ Cilamulo ca Yehova ndi cangwilo , cimabwezeletsa moyo . . . . Koma munthu woyamba Adamu , sanamvele Mlengi ndipo anataya mwai wokhala ndi moyo wamuyaya . 43 : 14 . Lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . Tili ndi mwai waukulu kwambili osati wodziŵa dzina la Mulungu cabe komanso woliimila monga “ anthu ochedwa ndi dzina lake . ” ( Mac . 15 : 14 ; Yes . Koma ngakhale n’conco , anthu ambili samvetsetsa cifukwa cake Yesu anafela mtundu wa anthu ndi mmene imfa yake ilili umboni wakuti Mulungu amatikonda . Iye anati uthenga wa Ufumu ‘ ukafesedwa paminga , . . . zilakolako za zinthu zina , zimaloŵa ndi kulepheletsa mawuwo kukula , ndipo sabala zipatso . ’ — Maliko 4 : 14 , 18 , 19 . Adani amenewa anagonjetsedwa pamene Yaeli , mkazi amene sanali waciisiraeli anapha Sisera , mkulu wa gulu la nkhondo la Akanani . — Ower . M’maiko a kum’maŵa ndi kumadzulo , tuakacisi twa m’nyumba ndi tumaguwa twa nsembe tumene anthu amapemphelelapo , kusinkhasinkha , ndi kupelekelapo nsembe . Motelo , dzifunseni kuti : ‘ Kodi ndimadya cakudya cotafuna ca kuuzimu ? 2 : 9 ) Kodi ndiye kunali kusintha kotsiliza ? Ayi . Munthu wacifundo amaona zosoŵa za ena na mavuto awo , amawamvela cisoni , ndipo amafuna kuwathandiza . Mwacionekele , Abulahamu adzasangalala kwambili m’paladaiso . Iye adzapitiliza kulimbitsa ubwenzi wake ndi Mulungu . Buku lina linakamba kuti : “ Ayuda anapatsidwa ufulu wambili m’boma la Roma . . . . Kodi kuganizila zamtsogolo kunamuthandiza bwanji Sara ? ( Salimo 37 : 29 ) Inunso mukhoza kukhala pakati pa “ olungama ” amene adzacha dziko lapansi mudzi wao kwamuyaya . [ Mau apansi ] Inde , abale na alongo otumikila ku gawo losoŵa akutiitana kuti , “ Conde , bwelani kuno ku Myanmar mudzatithandize ! ” N’nali Kukhulupilila Kuti Kulibe Mulungu 11 : 1 . 5 - 7 . Ganizilani za Yonatani , mwana wa Mfumu Sauli . ( 1 Akorinto 4 : 15 ; 2 Akorinto 2 : 4 ) Victor amene analela ana atatu anati : “ Zaka zimene ana anga anali acinyamata zinali zovuta . Ndikuthandiza ” Pita ukayanjane ndi m’bale wako coyamba . ” 4 - 6 . ( a ) N’cifukwa ciani timayamikila kuti Nowa ndi Mose anagwila nchito yao imene Yehova anawapatsa ? Panthawiyo zinaoneka zosatheka cifukwa Ababulo sanali kumasula akapolo awo . Kuti akafike bwino kumene akupita , amafunika kutsatila njila ya ndeke imene amuuza kuyendamo . Anafunika kukonzanso nyumba zowonongeka , kubyala mbewu m’minda , na kusakila zakudya . Ngati ticita zimenezi , zinthu zidzatiyendela bwino , ndipo Yehova adzakondwela kudziŵa kuti timayamikila cakudya cakuuzimu cimene watipatsa . — Yesaya 48 : 17 . Ngakhale n’conco , zithunzi zawo zingacititse anthu kulemekeza Yesu na ziphunzitso zake , kapenanso kumusuliza . Inamuthandiza maningi . Ambili a ise taonako zinthu zopanda cilungamo zicitika , anthu abwino ndi osalakwa kupondelezewa na anthu oipa . A “ nkhosa zina ” amathandiza Isiraeli wa kuuzimu pa nchito yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu . Anthu okhawo amene amacita zimenezi ndi amene adzaloledwa kukhala m’dziko latsopano limene Mulungu analonjeza . — Zek . N’zoona kuti cikondi ca pakati pa mwamuna na mkazi n’cofunika , koma cikondi cimene tikamba si cimeneci . Nanga Yehova anakambilatu za ciani ? Kodi anthu ena amakhulupilila ciani ponena za anthu amene amalambila Mulungu ? N’cifukwa ciani zimenezi zinali zofunika ? 2 : 16 - 18 ) Paulo anafotokozanso zinthu zina zimene zingatimanitse mphoto zimene zilipo ngakhale masiku ano . Mdani wathu Satana amaona nchito yaikulu yolalikila ndi kuphunzitsa za Ufumu imene ikucitika . Koma kodi munadzifunsapo kuti : ‘ N’cifukwa ciani anasankha kukatumikila ku dziko lina ? Kupatsa na mtima wonse kumathandiza kuti thanzi la anthu amene ali ndi matenda osatha , monga zotupa - tupa m’kati mwa thupi ( sclerosis ) kapena HIV , likhaleko bwino . Ngati mungathe , uzani akulu a mumpingo wanu ndipo apempheni kuti akuuzeni zimene muyenela kucita kuti muyambe utumikiwu . Pankhani yofuna kukhala mkulu , cofunika kwambili si ine , zimene ndifuna kapena malo amene ndifuna kutumikila . Takamba conco cifukwa kukonda coonadi kumatilimbikitsa kumvela na mtima wonse malamulo a m’Baibo akuti tizikonda Mulungu ndi abale athu . — 1 Pet . ( Gen . 32 : 26 - 28 ) N’zoona kuti kuŵelenga Baibo kumakhala kosangalatsa , koma sitifunika kuiŵelenga ngati buku la nthano . ( Luka 24 : 13 - 15 , 27 ) Pamenepo mitima yao inayamba kunthunthumila cifukwa anali ‘ kuwafotokozela Malemba momveka bwino . ’ — Luka 24 : 32 . Yesu anauza otsatila ake kukumbukila imfa yake osati kuukitsidwa kwake . ( Luka 22 : 19 , 20 ) — 3 / 1 , tsamba 8 . Kum’mwela kwa Lebanon konse anthu anali kundiopa kwambili pamene ndinali kumenya nkhondo yanga yothetsa kupanda cilungamo ndi nkhanza . ( b ) N’cifukwa ciani mfundo zili mu ndime 12 zingagwilenso nchito pankhani zina zaumwini ? N’zoona kuti cimapweteka ngati munthu wacotsedwa mumpingo , koma zotele zikacitika sitiyenela kutaya mtima . Pa nthawi ina , pafupi - fupi munthu mmodzi pa anthu atatu alionse mu ufumuwo anali kapolo . Kodi acinyamata oopa Mulungu angaphunzile ciani pa zimene takambilanazi ? Anthu ambili a m’Machalichi Acikristu amakhulupilila kuti , Akristu adzatengedwa ndi matupi ao . Koma ngati ana amaona kuti makolo awo amawakondadi , amalimbikitsidwa kuwamvela ngakhale pamene aona kuti n’zovuta kutelo . Conco , nthawi zambili abale anali kukhala na njala n’colinga cakuti agule Mabaibo . Koma kaamba ka zopeleka za ena zimene zikugwilitsidwa nchito m’njila yakuti “ pakhale kufanana , ” gulu la Yehova laseŵenzetsa ndalama zambili pocilikiza nchito yomasulila ndi kufalitsa Mabaibo . N’ciani cingatithandize kuona zofooka za anthu mmene Yehova amazionela ? Tifunika kukonda abale athu nthawi zonse , koma tifunikanso kukhala okonzeka kuwafela . N’zosacita kufunsa kuti iye anapemphela kwambili kwa Yehova kuti amuthandize kuyankha mwanzelu zimene angafunsidwe . Kodi tiphunzilepo ciani pa citsanzo cao ? ( Luka 2 : 46 , 47 ) Panthawi ina , pamene iye anali kulalikila , anagwilitsila nchito Mau a Mulungu mwaluso poyankha adani ake cakuti io anasoŵa zokamba . — Mateyu 22 : 41 - 46 . 2 : 11 - 14 ) Pa nthawiyo , Paulo anam’patsa uphungu Petulo , ndipo mwacionekele iye anaulandila . Ngakhale tilibe mavuto palipano , tidzakumanabe nao mtsogolo . Koma alongo amanikumbatila na kuniuza kuti naoneka bwino . “ Kumbukilani amene akutsogolela pakati panu . ” — AHEB . Ndiyeno , mlendoyo anakafunsa kuti , “ Nanga n’cifukwa ciani umasankha koini ya siliva ? ” Tiyeni tione zimene gulu la Mulungu la padziko lapansi likucita masiku ano otsiliza . Anthu ena amapemphela , koma amaona kuti sayankhidwa . Nimaona kuti unali mwayi waukulu kutengako mbali popititsa patsogolo nchito imeneyi . 1 : 15 - 17 , 20 , 21 ) Nthawi zina tingaganize kuti palibe amene amaona zabwino zimene timacita , koma Yehova amaona ndipo adzatidalitsa . — Mat . Iwo anakamba kuti pamene Sukulu ya Apainiya inayamba mu 1977 , ofalitsa anali kulimbikitsiwa kukatumikila kosoŵa . ( 1 Timoteyo 3 : 1 ) Koma Akristu onse angatengelepo phunzilo pa ziyeneletso zimenezi . Kuti muyambe kucita zimenezi , mungacite bwino kuyankha mafunso otsatilawa . Koma pambuyo poifufuza kwa miyezi itatu cabe , panabwela za mwadzidzidzi zimene zinasokoneza nchitoyo . Kulalikila ndi njila yabwino koposa imene tingaonetsele kuti tili ndi cikhulupililo . Ndi zinthu zabwino ziti zimene tingasinkhesinkhe ? Pamene anawasankha , anacititsa kuti asinthe kaganizidwe kao ndi ciyembekezo cao . Iye anacita zimenezi pogwilitsila nchito mzimu wake woyela . ( Yak . 1 : 1 ) Mwacionekele , sicinali covuta kwa Akhristuwo kulandila uphungu wake , cifukwa moni umene anawapatsa unaonetsa kuti nayenso anali kapolo mnzawo kwa Mulungu . Cifukwa ca dipo limeneli , timakhala otsimikiza kuti iye adzatikhululukila ndipo tidzapitilizabe kukhala mabwenzi ake . Kodi tingakhale na umoyo wotani ‘ tikaika maganizo athu pa zinthu za mzimu ? ’ Ndinayamba kukonda kwambili lemba la Salimo 73 : 28 . Ena amakayikila kuti Goliyati anali wamtali conco . 15 : 7 - 9 ) Kodi Yehova akanasankhadi mmodzi wa amunawo kutsogolela anthu ake ? Ndinali ndi mzimu wokonda dziko langa ndipo ndinali kukonda kugwila nchito . Conco , ndinayamba kuseŵenza nthawi yomweyo . ( Miy . 1 : 10 , 15 ) Ngakhale anzathu atitunthe bwanji , ni udindo wathu kupanga cosankha mogwilizana ndi cikumbumtima cathu cophunzitsidwa Baibo . Mukayamba kuigwila bwino nchito imene mwapatsidwa , muzionanso mbali zimene mungaongolele kuti ulendo wotsatila mukaicite bwino kwambili komanso mwamsanga . Pasanapite mawiki aŵili , ophunzila a Yesu anafufuza m’Malemba ndi kupempha citsogozo kwa Mulungu . Ndiyeno anasankha Matiya kuti aloŵe m’malo Yudasi Isikarioti kukhala mtumwi wa namba 12 . ( Mac . 20 : 1 - 5 ) Koma panthawiyi , zinthu sizinamuyendele bwino Mose . Kodi Malemba amaonetsa bwanji kuti pangano la Abulahamu lidzakwanilitsidwa kwakukulu mtsogolo ? Nanga zimenezo zimatikhudza bwanji ? Pamene mngelo wa Yehova anacenjeza Yosefe kuti Mfumu Herode ifuna kupha Yesu , Yesu na makolo ake anathaŵa n’kukhala ku Iguputo . Cipembedzo Coona , — September - October mu Nsanja ya Olonda ya October 15 , 1995 . N’ciani cinathandiza Anna mkazi wamasiye kukhala wacimwemwe ? Anthuwo anali aubwenzi , opembedza ndipo anali kuidziŵa bwino Baibulo . ( 2 Mbiri 16 : 9 , 10 ; 24 : 18 - 22 ) Komanso sanali kubisa olo zolakwa za iwo eni , ndi za atumiki ena a Yehova . Yakobo anafunsa kuti : “ Kodi pakati panu pali aliyense wanzelu ndi womvetsa zinthu ? Izi zinaonetsa kuti Yehova sadzalola kuti anthu ake akagwidwenso ukapolo na Babulo . Ngati muŵelenga Baibo imene ili na mau ambili ovuta kumva , acikale , kapena amene simuwadziŵa , simungakondwele poiŵelenga . Pelekani citsanzo cimodzi ca zinthu zopanda cilungamo zimene Ayuda anali kucitilidwa m’nthawi ya atumwi . Pamene Yesu anati , “ mmene Atate wanga wacitila pangano la ufumu ndi ine , ” mwacionekele anali kukamba za pangano limene Yehova anapanga ndi iye kuti akhale “ wansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melekizedeki . ” — Aheb . Tiyeni tikambilane mfundo zazikulu ziŵili . Zinthu zonse zisanaonongedwe kothelatu padzikoli , Mulungu adzalowelelapo kuti aononge anthu amene akuonoga dziko lapansi . Mwacitsanzo , Baibulo limaticenjeza pa zinthu zimene zingaononge maganizo ndi matupi athu . Conco , timapewa kukoka fodya kapena kuseŵenzetsa mankhwala osokoneza bongo . 15 : 20 ) Ndani amacititsa citsutso cimeneci ? 39 : 21 - 23 ) Panthawi yovuta imeneyo , Yosefe anayembekezela moleza mtima kwa Mulungu wake . Gulu la acinyamata oledzela linapha mwankhanza mtsikana wa zaka 9 ndi kumenyanso bambo ake ndi msuweni wake . 15 , 16 . ( a ) Kodi ndi zinthu zocititsa cidwi ziti zimene zidzacitika mkati mwa Ulamulilo wa Zaka 1,000 ? 7 Kufunafuna Cuma Ceni - ceni Ngati muli ndi makolo amene amakonda Yehova naonso angakuthandizeni . Koma onani zimene mneneli Yesaya anakamba . Asilikaliwo anafuula kuti , ‘ Coka pamene wabisalapo ! ’ Ndimakondwela kwambili ndikakumbukila nthawi imene tinali kulalikila pamodzi . M’nkhani yaciŵili , tidzakambilana zimene tingacite kuti tikhale anthu auzimu ndi mmene kukhala munthu wauzimu kungatithandizile mu umoyo wathu wa tsiku na tsiku . Malemba amati : “ Poona cikhamu ca anthu , iye anawamvela cisoni , cifukwa anali onyukanyuka ndi otayika ngati nkhosa zopanda m’busa . ” Ndipo ena amakamba kuti , “ Ndimacita mantha kuyamba kuphunzila Baibulo . ” Iwo amanena kuti kusagwilizana kwa zipembedzo ndiye kwabweletsa mavuto amene alipo masiku ano . Asanayambe kuyenda ndi Yesu , atumwi ena anali asodzi a nsomba m’nyanja ya Galileya . Tingapindule bwanji ndi fanizo la mwana wolowelela ? Kusintha kumeneku kunanenedwelatu mu ulosi wa m’Baibo . Kodi ubwenzi wa Yehova ndi Abulahamu unasiyana bwanji ndi ubwenzi umene Yehova anali nao ndi Aisiraeli ? Ni cenjezo lanji limene Yehova anapeleka pa za ciwonongeko ca Yerusalemu ? Nanga n’ciani cinali kudzacitikila Ayuda ? Mexico 800,000 Iye anati : “ Ndinasangalala kumvetsela makambilano olimbikitsa a alongo aŵili amene anayenda ulendo wa pa boti kucokela ku Europe . ” Mungaonetse bwanji ana anu kuti mumawakonda ? ( Yobu 27 : 5 ) Komabe , kwa kanthawi , Yobu analeka kuona zinthu moyenela . Tiyeni tikambilane njila zitatu za mmene tingacitile zimenezi . Yesu ndi atumwi ake sanali kugwila nchito kuti apeze ndalama zodzithandizila pa nchito yao yolalikila . Mayankho aafupi na ocokela pansi pa mtima opelekedwa ndi ana , acititsa anthu ena acidwi kuzindikila kuti timaphunzila coonadi . — 1 Akor . Ndimapemphela kuti anthu mamiliyoni aphunzile Baibulo , alandile coonadi , ndi kutumikila Yehova mogwilizana ndi gulu la abale la padziko lonse . ( 1 Pet . Kodi pali amene angadziŵe ? Timalengeza kuti iye anaikidwa kukhala Mfumu ya Ufumu wa Mesiya kumwamba . Nanga linali kusiyana bwanji ndi mpukutu ? Kodi dzuŵa limakwanitsa bwanji kutulutsa mphamvu ya kutentha na kuwala ? Tsiku na tsiku iwo amaona kapangidwe ka luso ndi kodabwitsa ka zinthu , ndipo zimenezi zimaŵapatsa umboni wakuti amene anapanga zinthu zimenezo ni wanzelu kwambili , osati zakuti zinakhalako zokha . Kodi fanizo la Yesu la wofesa mbewu amene amagona limatanthauza ciani ? Ndinakhulupilila zimenezi , ndipo ndinaganiza kuti ngati apapa amene Akatolika amawaitana kuti Atate Woyela , amenenso ziphunzitso zao n’zodalilika , amakamba kuti ciphunzitso ca Utatu n’coona , ndiye kuti n’coonadi . Ponena za kuuka kwa akufa , kodi Baibo imaonetsa kuti n’ciani cidzacitika m’nthawi ya kukhalapo kwa Khristu ? Iye anafunika kusankha , kaya kuthandiza munthu woipa ameneyu kapena kukhala ku mbali ya Yehova ndi kupha mdani wa anthu Ake . Aliyense adzaziyankhila mlandu pamaso pa Woweluza wolungama , Yesu Kristu , amene wasankhidwa ndi Yehova . Anathetsa kulambila mafano ndi kukhulupilila mizimu m’dzikolo , ndipo analimbikitsa anthu kuti azimvela Yehova . N’cifukwa ciani tiyenela kusamala ndi zinthu zimene dzikoli limafalitsa ndi kuulutsa ? Ambili amaniitana kuti Amama kapena Ambuya . Moyo unali wovuta kwambili ndipo upandu ndi nkhanza zinafika pacimake . Nthabwala ndi zabwino ndipo zimakometsa nkhani . Ndipo mumadziŵa bwino kuti nthawi zina , apainiya ndi ofalitsa amakumana ndi mavuto amene angacepetse cangu cao mu utumiki . Komanso , pali ma IUD okhala na mahomoni . Mtundu umenewu unayamba kugwilitsidwa nchito mu 2001 . Cikondi cathu pa iye cidzalimba kwambili pamene tidzakambitsilana yankho la funso limeneli m’nkhani yotsatila . Kudzipenda moona mtima kumeneko kunam’limbikitsa kusamukila ku Ghana kuti awonjezele utumiki wake . Pamene Rubeni anacita colakwa , udindo monga woyamba kubadwa unacoka kwa iye n’kupita kwa Yosefe . ( Gen . Coyamba , Mauthenga Abwino analembedwa zaka pafupifupi 2,000 zapitazo . Posapita nthawi , iye anazindikila kuti ziphunzitso zambili zimene zili m’machechi osiyanasiyana si zipezeka m’Baibulo . Anthu ambili amene sanali Aisiraeli anakhala mbali ya mtundu wobadwanso wa Ayuda , ndipo patapita nthawi anthu ena akunja anatengela zikhulupililo za Ayuda . Komabe , Baibulo limakamba mosapita m’mbali kuti , “ Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu , ndipo ndi opindulitsa . ” Koma zinthu zitasintha , Mboni zimenezo sizinaphedwe . DAVIDE anayesetsa kudzilimbitsa kuti asilikali amene anali kuthawa adani asamukankhe n’kumugwetsa . Kodi iye amacitila dala kuti anikhumudwitse ? Mwacitsanzo , nkhani yosankha zosangulutsa ingayambitse “ mafunso opusa ndi opanda nzelu . ” Ndiye cifukwa cake bungwe la mgwilizano wa zipembedzo limadzicha kuti ndi “ bungwe lolimbikitsa mgwilizano , ” osati gulu lacipembedzo . Cifukwa ca mzimu wa mpikisano masiku ano , anthu ambili amacita zinthu n’colinga cakuti adziŵike . 16 , 17 . ( a ) Kodi Mboni za Yehova zimakondwela kuona ciani m’maiko ambili ? Pasanapite nthawi yaitali , zinthu zinayamba kusintha . Kuphonya pa Kamvedwe , Na . Nanga ndikanafuna kuti wina andicitile ciani ? ’ — 1 Pet . Patangopita nthawi , dziko la Britain linayamba kuphulitsa mabomba . Ni nkhani yaikulu iti imene Paulo anakamba pa Aroma 8 : 4 - 13 ? caputala 40 6 : 10 , 11 . 4 : 11 , 12 ; 2 Tim . 1 : 1 , 2 , 7 ) Komabe , patapita zaka 10 , iye anasintha cakuti Paulo anauza mpingo wa ku Filipi kuti : “ Ndikuyembekeza kutumiza Timoteyo kwa inu posacedwapa . . . Ife tonse tifunikila malangizo ndi uphungu wocokela m’mau a Mulungu . Zakuthambo zinalinganizidwa mwadongosolo lodabwitsa ngako . Kodi mphatso ya mtendele imeneyi imatithandiza bwanji kubala zipatso ? Tiyeni tibwelele kumbuyo zaka ziŵili kapena zitatu mumzinda wa Lusitara , kumene Timoteyo anali kukhala . Kusinkhasinkha pa mfundo zimene zili m’kabokosi kameneka kungakuthandizeni kupitiliza kulalikila mwacangu . Ndiyeno , analamula kuti Baibo ya Malemba a Cigiriki imene iye anamasulila iwochedwe poyela , ndipo anakambanso kuti zolemba zake zina zinali “ kulimbikitsa mpatuko wa Luther . ” Tidzaphunzila mmene mphamvu yotha kuganizila zinthu zimene sitinazionepo ingatithandizile kukhala ndi cikhulupililo colimba , ndi kutsanzila makhalidwe a Yehova monga cikondi , kukoma mtima , nzelu , ndi cimwemwe . Ofufuza apeza kuti anthu amene amakondetsetsa kutamba zamalisece , amalephela kudziletsa mofanana ndi anthu amene amamwa mowa mwaucidakwa ndi amene amaseŵenzetsa mankhwala osokoneza ubongo . Conco , n’zosadabwitsa kuti kutamba zamalisece kumakhala na zotulukapo zoipa . Mwa ici , tinali kusiyana maganizo na kukhumudwitsana nthawi zina . Ngati n’conco , zitsanzo za Nowa , Danieli , na Yobu zingakulimbikitseni . 60 : 13 ) Kodi iye amacita bwanji zimenezi ? 11 , 12 . ( a ) Kodi Mfumu yatsopano inayamba kucita ciani pambuyo pankhondo m’caka ca 1919 ? ( Aheberi 10 : 12 , 13 ) Yesu anafotokozela ophunzila ake mmene angadziŵile kuti nthawi ya kuyembekezela yasila , ndi kuti wayamba kulamulila kumwamba . Yobu anafunsa funso lofanana ndi limeneli pamene anaona kuti ali pafupi kufa . Mu 1881 , magazini ya Zion’s Watch Tower inakamba kuti “ Mwana wa munthu ” kapena kuti “ Mfumu ” ndi Yesu . Sindikonda yogati . 25 : 1 - 12 ; 26 : 1 - 3 . Cimene tapangaco n’cosankha inde , koma cikhoza kutigwetsela m’mavuto . ( Kudziŵa cifukwa cake kutithandiza kukhala omvetsa zinthu . ) M’kupita kwa nthawi , ndinadziŵa kuti io anatumikila monga Mboni zonyamula mabuku mwakabisila , pamene nchito yolalikila inali yoletsedwa ndi cipani ca Nazi ku Germany . Conco , anthu angaonetse makhalidwe a Mulungu . Kodi Paulo anacenjeza Agalatiya za ciani ? Mkulu wa asilikali anaika Yosefe kuti azilondela amuna aŵiliwo amene poyamba anali ndi udindo wapamwamba . ( 1 Yoh . A Zimba : O - oo , ndikumvetsa tsopano , mutanthauza kuti nthawi zokwanila 7 zinatha mu 1914 ? Ndinazindikila kuti a Mboni amapangadi gulu lonse la abale padziko lapansi . 21 : 2 , 9 - 14 ) Mulungu akamakamba kuti amakonda ana ake a kuuzimu m’Baibulo , mumtima mwanu mumati , “ Akukamba za ine . ” 13 : 43 . ( b ) Kodi kudziŵa mphamvu za Satana kuli na ubwino wanji ? Ni “ kuuka kwabwino kwambili ” kuti kumene kudzacitika m’tsogolo ? Ndiyeno , m’miyezi yotsatila nkhani za m’Baibulo zinali kupelekedwa m’tauni ya Kyoto ndi m’matauni ena a kumadzulo kwa Japan . BAIBULO limatilamula kuti tizimvela maboma a anthu , koma limanenanso kuti tiyenela kumvela Mulungu nthawi zonse . Pa nthawi ina , Eliya anali kuganiza kuti panalibe wina aliyense amene anali kutumikila Mulungu mokhulupilika kupatulapo iye ndipo mwacionekele anali kufunitsitsa kukumana ndi Elisa . — 1 Mafumu 18 : 22 ; 19 : 14 - 19 . 31 : 29 , 30 ; 32 : 28 , 29 . N’cifukwa ciani Yehova anapulumutsa Nowa ndi Rahabi ? N’nayamba upainiyawo pa 1 January , 1952 , pamene n’nali ndi zaka 15 . Kumeneko analengeza zakuti tinacita ngozi , ndipo abale mokoma mtima anatipatsa ndalama . Mtumwi Paulo analimbikitsa Akristu kuti : “ Pitilizani kudziyesa kuti muone ngati mukadali olimba m’cikhulupililo . Atate anamwalila pamene n’nali na zaka 8 . Pamene Marilyn anaganiza zobwelela kunyumba , anthu ena anam’limbikitsa kubwelela koma ena sanatelo . Mukamagwila nchito mofunitsitsa , mumakhala acimwemwe pa nchito yanu . ( Mat . 26 : 26 , 27 ) Mkate ndi vinyo anali ndi tanthauzo lapadela . Ndipo Yesu anaphunzitsa atumwi ake okhulupilika zinthu zambili pausiku wosaiwalikawo . Conco , tiyeni tigwilizane ndi zolengedwa zokhulupilika za kumwamba pokamba kuti : “ Mulungu wathu wanzelu , wamphamvu ndi wa nyonga , atamandidwe , apatsidwe ulemelelo ndi ulemu , ndipo ayamikilidwe kwamuyaya . ( 2 Mbiri 20 : 13 ) Onse pamodzi , acicepele ndi acikulile , anakhulupilila Yehova ndi kutsatila malangizo ake , ndipo Yehova anawateteza kwa adani ao . Koma bwanji ngati thanzi lathu likufookela - fookela ? 4 : 6 , 7 . Conco , pewani kutumila mwamsanga uthenga kwa aliyense amene mumadziŵa . Aphunzitsi anga anaona kuti ndinali ndi luso lovina , ndipo anayamba kundiphunzitsa maluso ambili a kavinidwe . Kodi zinali zotheka kuti munthu wangwilo akhale wokhulupilika kwa Yehova akayesedwa ndi “ woipayo ” ? Kunja kunali kotentha kwambili cakuti m’ndende munali ngati m’ng’anjo yamoto . Ndiyeno , ndinapempha ofesi ya nthambi kuti ndikatumikile kumwela kwa dziko la Japan pafupi ndi acibale anga kuti Amai asamade nkhawa kwambili . ( a ) Kodi ubwenzi wa Mose ndi Yehova unali wolimba motani ? Anawauza kuti : “ Ine ndidzakusenzetsani goli lolemela kwambili , ndipo ndidzawonjezela goli lanulo . Anchito odzipeleka amene akugwila nchito yomanga ku Warwick Ngakhale kuti asilikali ambili anali kufa , akulu - akulu a asilikali anakakamizabe anthu ao kukamenya nkhondo yoopsayo . Inali nthawi ya m’madzulo . Kodi tingasankhe kucita ciani pankhaniyi ? KUMAMATILA kwa Yehova n’cinthu canzelu . Conco , mau otsiliza a Mose analimbikitsa Aisiraeli kucita zimenezo . Yury ndi Oksana akucita upainiya wapadela . Ngakhale kuti munthu wadziŵa “ ciphunzitso coyambilila ca Khiristu , ” afunikabe kucita khama kuti apite patsogolo . ( Aheb . Ndinali kulephela kucitako nthabwala cifukwa cosadziŵa cinenelo . ” Conco Mose anaigwila , ndipo inasandukanso ndodo m’dzanja lake . ( Ŵelengani Masalimo 83 : 18 . ) Nanga bwanji za ana ambili amene anathaŵa kwawo kapena kusamukila ku mayiko ena pamodzi na makolo awo ? Tisadelele zimene tingakwanitse kucita pogwila nchito ndi Mulungu mwa kucitila umboni za dzina lake ndi kulengeza za Ufumu wake . Koma Yehova saona kuti munthu wina kapena gulu lina la anthu ndi labwino kuposa lina . Koma sindikaikila kuti Yehova amandikonda cifukwa ananditsogolela ngakhale pa nthawi zovuta kwambili . Sanandilole kuti ndiyesedwe kufika pamene sindingapilile . ” ( 1 Akor . Koma kumatanthauza kuti nkhani ziŵilizi , ya ulamulilo wa Mulungu ndi ya cipulumutso , timaziona moyenelela . Tsiku lotsatila , Samueli anadzoza Sauli , anamupsompsona , ndi kumupatsa malangizo oonjezeleka . Kodi mungamvele bwanji ngati anthu akana kukulembani nchito ? Mwacitsanzo , pamene khamu la anthu linali ndi njala , Yesu anapemphela ndi kudyetsa khamulo m’njila yozizwitsa . 26 : 4 . Naomi anali kudziŵa kuti umoyo wa ku Betelehemu udzakhala wosiyana kwambili ndi umene Rute anazoloŵela . Mkaziyo anali ndi mphatso yapadela yodzabeleka ana . N’zosatheka kuti wina mu mpingo mwadala ayambe kulambila mwacinyengo . Ndipo n’zoona adzauonadi . Iye wakhala m’cikwati kwa nthawi yaitali , ndipo adziŵa kuti mwamuna wake amafuna kuti iwo azigwilitsila nchito ndalama mosamala . 56 : 8 ) Ndinayamba kuganizila mozama za ciyembekezo ca ciukililo , ndipo mtima unakhala pansi . Nthawi zonse , Yehova amatsogolela anthu ake . Anita anawonjezela kuti : “ Nthawi zina , mokondwela nimauza alongo acicepele kuti , ‘ Iwenso nyamula cola cako , ukatumikile kudziko lacilendo . ’ Conco , n’naganiza zakuti mwezi uliwonse nizicita zimenezo ndipo n’napitiliza mpaka zaka pafupi - fupi zitatu . Mu 1978 , ndinabwelela ku Los Angeles kukasamalila amai cifukwa anali kudwala . Onani Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 , tsamba 16 - 18 , ndime 5 - 8 , 12 . ( Afilipi 2 : 13 ) Pemphelo lathu n’lakuti Yehova apitilize kutipatsa mphamvu zokwanila kuti tizicita zimene tingathe polalikila uthenga wabwino . — 2 Timoteyo 4 : 5 . Yesu nayenso wakhala akuyembekezela moleza mtima . Kuzungulila dziko lonse lapansi , anthu a zinenelo na zikhalidwe zosiyana - siyana amakamba nkhani zokhudza paradaiso . Matupi a nyama a odzozedwa amene adzakhala ndi moyo panthawiyo sadzatengedwa kupita kumwamba . Baibulo limafotokoza mmene cinyengo cinayambila . Limatiuza kuti cinyengo cinayambila kumwamba ndi colengedwa cauzimu osati anthu . Kodi Yehova amawaona bwanji anthu amene amaziona kuti ndi ofooka mu mpingo ? Ngati anthu sakhulupilila nsembe ya Yesu , Mulungu amawaona kuti ni adani ake . Mwina anali kuyembekezela mwacidwi nthawi imene adzalandila abale ao kapena mabwenzi ao amene adzaukitsidwa . Zipembedzo zambili zimakumana pamodzi kuti zigwilizane pa mfundo imodzi ndi kulimbikitsana . Ndinadziŵa kuti Mulungu amadana ndi zinthu zopanda cilungamo ngakhale kuti amalola kuti zizicitika , ndipo adzazicotsapo posacedwapa . Mipukutuyo idzatithandiza kumvetsa maganizo a Yehova . Mtumwi Petulo anaticenjeza kuti sitiyenela kuona ufuluwu monga mwayi wokhutilitsila zilakolako zathu za thupi . Mwacitsanzo , posacedwapa m’mipingo yambili , abale ndi alongo anali kuphunzila buku lakuti Yandikirani kwa Yehova pa Phunzilo la Baibulo la Mpingo . Cosankhaco cidzakonza tsogolo lanu lonse . — Sal . Ngakhale kuti mtumwi ameneyu zikanam’vuta kupitilizabe kucita bwino kuuzimu , Yesu anafunabe kum’gwilitsila nchito kuthandiza ena . Mosayembekezela , ambuya aamuna anavomeleza . Tonse tinali atumiki othandiza ndipo tinali kusangalala kutumikila pamodzi . Ngati tiwaonetsa cikondi ndi kuwathandiza , cikhulupililo cawo cidzalimba . — Miy . Mneneli Natani anakhalabe wokhulupilika kwa Yehova ndiponso kwa Davide . Ni makonzedwe anji amene Aisiraeli anapanga okhudza kuimba polambila ? Annie anapitiliza kuti : “ Alongowo anali osangalala kwambili pamsonkhanopo . Maakaunti Akubanki : Ngati n’zovomekezeka kwanuko , mukhoza kupeleka zinthu monga maakaunti anu akubanki , zikalata zosungitsila ndalama , kapena maakaunti a ndalama zimene mukusunga kuti mudzagwilitse nchito mukadzapuma pa nchito . Ngakhale pamene tinasoŵelatu cocita , iye anatilimbitsa ndi kutipatsa thandizo limene tinali kufunikila . ” Pokambilana , colinga canu cikhale kukhazikitsa mtendele . Kenako adzaona Mwana wa munthu akubwela mumtambo ndi mphamvu ndi ulemelelo waukulu . ” Na ise tingapeze madalitso monga amenewa ngati tiyesetsa kupita patsogolo mwauzimu . GWILITSILANI NCHITO BAIBULO KUTI MUONE NGATI NDINU WODZIKONDA Kodi Yehova ali nawo colinga canji anthu ? ( Mat . 5 : 43 - 45 ) Mtumwi Paulo anakamba mfundo yofananako pamene anati : “ Ngati mdani wako ali ndi njala , um’patse cakudya . Yehova ni Mlengi . Adamu na Hava anali na ufulu wosankha kumvela Mulungu kapena kusamumvela . ( Yoh . 5 : 28 , 29 ) Kodi lonjezo limeneli limathandiza bwanji mwamuna kapena mkazi amene wafeledwa ? Yehova amatifunila zabwino . Gulu la Yehova lapanga masinthidwe otani m’zaka zaposacedwapa ? Ana anga ndi azikazi awo . Mwacitsanzo , Levitiko macaputa 13 na 14 afotokoza malamulo amene anapatsidwa kwa Aisiraeli okamba za ukhondo na kupatula anthu odwala matenda oyambukila . Kuphunzila Baibo pogwilitsila nchito Nsanja ya Mlonda ndiyo njila yaikulu imene Mulungu amatiphunzitsila . ( Gen . 3 : 1 - 6 ) Hava anaona kuti zimene Satana anamuuza zinali zabwino . Ndiye cifukwa cake Yesu anati : “ Yekhayo amene adzapilile mpaka pa mapeto ndi amene adzapulumuke . ” — Mat . Iye anati : “ Khalani maso . ” Kamodzi pacaka , Maria anali kubwela ku Saransk kudzaniona ngakhale kuti ulendo wa pa sitima kucoka ku Tulun ndi kubwelela , unali kutenga masiku 12 . Cimakwilila zinthu zonse , . . . cimayembekezela zinthu zonse , cimapilila zinthu zonse . ( b ) Tidziŵa bwanji kuti lemba la Salimo 16 : 10 silinakwanilitsike pa Davide ? Kukamba zoona , ubatizo ndi cosankha cacikulu . Nanga Yehova anacitanji ndi zimene Satana anatsutsa mu Edeni ? Iye ndi munthu woyamba kuchulidwa m’Baibo kuti anayendabe ndi Mulungu . Nimakonda kupita kwa munthu amene wakhala pansi m’Nyumba ya Ufumu , amenenso sakukamba na aliyense kuti nikambe naye . Ponena za miyezo yapamwamba imeneyi , m’bale wina dzina lake Raymond , amene watumikila monga mkulu kwa zaka zambili anati : “ Cinthu cacikulu kwa ine ndi kukhala mmene tilili . Pamene Yesu anali kubadwa , mkazi wamasiye ameneyu anali ndi zaka 84 . MAPHUNZILO A BAIBULO 2 : 9 , 16 , 17 ; 3 : 1 - 6 . Mau amene Davide anakamba ponena za mmene iye amatikhululukila , amaonetsa kuti tilidi ndi Atate wacifundo . Davide anati : “ Tamanda amene akukhululukila zolakwa zako zonse , iye amene akukucilitsa matenda ako onse . Akristu a m’nthawi ya atumwi anali kutsatila citsanzo cimeneco , ndipo ifenso timatsatila citsanzo cimeneco . Mtsogoleli wa dziko la Germany anati : “ Tikumenya nkhondo kuti titeteze zinthu zathu , miyambo ndi cikhalidwe cathu ndi kukonza tsogolo lathu . ” Paulo analemba kuti , “ Mulungu akuonetsa cikondi cake kwa ife , moti pamene tinali ocimwa , Kristu anatifela . ” Timamvetsetsa mmene anali kumvelela akakhumudwa , akacita mantha ndiponso akalakwitsa zinthu . Ise Akhristu tiyenela kutengela Yehova , osati Afarisi . Ndipo “ ndi amphamvu ” motani ? Ngati n’conco , pemphani Yehova kuti akuthandizeni kuthetsa mantha . Ku Yangon m’dziko la Myanmar , ophika anali kucita zinthu moganizila ena . Iwo anali kuika mphilipili yocepa m’zakudya za alendo ocoka m’maiko ena . Lemba la Aroma 12 : 15 limati : “ Lilani ndi anthu amene akulila . ” Inde , monga Paulo , tingapitilize kubala zipatso mopilila . Tiphunzilapo ciani pamenepa ? Ngakhale kuti anthu amene anali kufuna kukhutilitsa zilakolako zao zinthu zinali kuwayendela bwino , Mose anali kukhulupilila kuti oipa adzaonongedwa . Ali yekha m’cipululu , Eliya anayamba kuganiza kuti nchito yake monga mneneli inali yacabe - cabe . Timaona izi ndi mmene anali kupelekela cilango kwa Aisiraeli , amene anam’pandukila mobweleza - bweleza . Anati : “ Ndithu ndikukuuza lelo , Iwe udzakhala ndi ine m’Paladaiso . ” — Luka 23 : 39 - 43 . 1 : 33 . 7 : 6 - 8 ) Uku sikunali kungosankha cimene wakonda cabe ayi . Conco , tisaganize kuti kukali nthawi yaitali kuti “ Nyanga 10 , komanso cilombo ” zochulidwa pa Chivumbulutso 17 : 16 ziukile Babulo wamkulu amene ndi ufumu wa dziko lonse wa cipembedzo conama . Ngakhale m’masiku ano otsiliza a dongosolo la Satana , Yehova amadalitsabe anthu ake . Ndipo cimene cinacititsa kuti Yudasi Mgalileya , amene tamuchula poyamba paja , aukile ulamulilo wa Roma ni kukhazikitsidwa kwa lamulo lakuti Ayuda azipeleka msonkho kwa Aroma . Popeza anali atalaŵa Mau a mulungu na kumvela kuwama kwake , mtima unali dyoko - dyoko kufuna kuphunzila zambili ! Pa nthawi inayake Babulo Wamkulu akadzaonongedwa , Yesu adzasonkhanitsa Akristu otsalila onse amene ali m’gulu la mkwatibwi . ( 1 Ates . 24 : 13 ; Maliko 3 : 14 ) Kugwila nchito imene Yesu anawapatsa kunali na zovuta zake . Koma iwo anakwanitsa kugwila nchitoyo na kukhalabe mabwenzi ake . Kuti tipeze mayankho a zoona a mafunso awa , tiyenela kukamba nawo abale ndi alongo amenewa . Mfundo imeneyo yazikidwa pa mbali ziŵili . Koma anakhulupilila kuti Yehova adzam’tonthonza . M’maganizo mwanga , ndinali kumva ndi kuona anyamata akundifunsa kuti , “ Kodi ndidzacila ine ? ( Genesis 18 : 6 ) “ Ufa wosalala ” umene Sara anagwilitsila nchito uyenela kuti unapangidwa ndi tiligu wocedwa emmer kapena unapangidwa ndi barele . Tidzaphunzilanso za kaimidwe kolimba kamene Ophunzila Baibo anatenga kulinga kwa Babulo Wamkulu . Tidzaonanso kuti n’liti pamene Akhiristu anamasuka mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu . N’ciani cimene anthu akufunikila kwambili ? Tiyeni titengepo phunzilo lakuti , ngakhale nkhani zokhudza banja , monga cikwati kapena kulela ana , zisatiiŵalitse mfundo yakuti tsiku la Yehova lili pafupi kwambili . ( 1 Maf . 8 : 27 , 29 ) Ayuda atabwelela kwao kucokela kuukapolo ku Babulo , anali kusonkhana nthawi zonse m’masunagoge . ( Maliko 6 : 2 ; Yoh . 18 : 20 ; Mac . Zimenezo zinatikwiitsa kwambili cakuti tili mu holo yoonetsa masewela , tinamenya ndi kuvulaza anyamata a ciyela . Tili na cimwemwe cifukwa ca zitsanzo zabwino zimene anatisiila , ndiponso cifukwa ca citsanzo cabwino cimene tayesetsa kusiila ana ndi adzukulu athu . Ngati munthu ni wacifundo , amakhala kholo labwino , mkazi kapena mwamuna wabwino , ndiponso bwenzi labwino . Mwacitsanzo , ana ena amaphunzila kupeleka ndemanga , kucita zitsanzo , ndi kukamba nkhani m’citundu ca makolo awo , koma zimene amakamba sizikhala zocokela pansi pamtima . Anthu ena mumpingo anali kulimbikitsa ziphunzitso zampatuko . N’zifukwa ziti za m’Malemba zimene zimatilimbikitsa kupitiliza kulalikila ? 5 Kodi Muli na Mngelo Wokutetezani ? Mulungu anafuna kuti io akhale ndi cikwati cacimwemwe , ndi kuti adzadze dziko lapansi ndi ana . Ngati mwininyumba wavomela kumvetsela , wofalitsa anali kutsegula nkhani yaifupi yojambulidwa , ndipo pamapeto pake anali kumugaŵila zofalitsa . Ganizilani zimene zinacitikila Sakura * wa ku Japan . Mosasamala kanthu ndi cizunzo ca nkhanza cimene Mboni zinakumana naco ku Europe , izo sizinaiŵale nchito yao yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu wa Yehova . Mfundo yakuti Mulungu amasankhilatu mayeselo amene tidzakumana nawo ionetsa kuti afunika kudziŵa zonse zokhudza tsogolo lathu . Zimene Adamu na Hava anasankha kucita zinabweletsa mavuto ambili ( Onani palagilafu 9 - 12 ) ( Aheb . 11 : 26 ) Ngakhale kuti Mose sanadziŵe zambili zokhudza zinthu zamtsogolo , iye anapanga zosankha mogwilizana ndi zocepa zimene anali kudziŵa . Kodi tingaonetse bwanji kuti timakonda Mulungu ? Iwo anali kusonkhezela anthu kuti aziona Yesu monga kalipentala wamba ndiponso ophunzila ake monga “ osaphunzila ndiponso anthu wamba . ” ( Mac . ( Yoh . 10 : 16 ) Ngakhale kuti a nkhosa zina ndiponso odzozedwa ali ndi ziyembekezo zosiyana , io amalambila Yehova mogwilizana pano padziko lapansi . Tiyeni tikambilane zifukwa zinayi zimene zatifikitsa pa mfundo imeneyi . 50 : 19 , 20 ) Pamapeto pake , Yosefe anaona kuti anacita bwino kuyembekezela Mulungu . Iye anali kucitanso maulendo aubusa ambilimbili . KAPEPA koitanila anthu ku Cikumbutso n’kamodzi mwa zofalitsa zambili zimene timapulinta caka ciliconse . Conco , sangayenelele kutumikila pa udindo uliwonse kapena kupatsidwa utumiki uliwonse wapadela mumpingo . Kodi lemba la Aroma 14 : 13 , 19 limakhudza bwanji cosankha cathu pankhani ya thanzi ? N’kofunika kuganizila mmene timalankhulila ndi zimene timalankhula . Kodi Kuukitsidwa kwa Yesu Kumatanthauza Ciani kwa Ife ? Mwathandizo la Yehova , n’naleka kutamba za malisece m’kupita kwa nthawi . Kukhala na mwayi wothandiza anthu aconco kudziŵa Yehova , kumanicititsa kukhala na cimwemwe coculuka . ” Nkhaniyo inafotokoza kuti “ Ufumu wa Mulungu udzabwela kudzaononga dziko la Satana osati dziko lapansili . ( Onani cithunzi pamwamba . ) ( b ) Kodi anthu a Mulungu amalandila malangizo otani amene angawapulumutse ? Julie nayenso anati : “ Sitinakhalepo ndi cimwemwe cimene tili naco , ndipo ndife okhutila cifukwa ca zimene tacita . Mwacitsanzo , ku Roma , akapolo anafunika kugwila nchito m’migodi kwa zaka pafupi - fupi 30 . 3 : 5 , 8 - 10 . Yehova amatetezabe anthu amene amam’khulupilila ndi kum’dalila monga mmene Debora , Baraki ndi asilikali olimba mtima aciisiraeli anacitila . Nkhondoyo itatha , asilikali anabwelela kwao . Koma popeza kuti anali asanacile matendawo , io anafalitsa mliliwo mwamsanga padziko lonse . Tingaucilikize mwa kukhala wokhulupilika , kucita utumiki wathu ndi mtima wonse , ndi kucita zonse zotheka kuti titengele citsanzo ca Mulungu pa zilizonse zimene timacita paumoyo . Tingatsimikize bwanji kuti Yehova amadziŵa kuti munthu wofedwa afunika citonthozo ? Kale , ziyamikilo zonse zokhudza kuika akulu ndi atumiki othandiza pa udindo zinali kutumizidwa ku ofesi ya nthambi ya m’dzikolo . ( Sal . 87 : 1 , 2 ) Udindo wa Yesu m’makonzedwe a Yehova umanenedwanso kuti maziko . ( 1 Akor . 3 : 11 ; 1 Pet . Kuona zolakwa moyenela kudzatithandiza kuyankha mafunso amenewa . Paulo , polembela Akristu a ku Korinto , anagwilitsila nchito mau akuti “ zofooka ” ndi akuti “ wofooka ” ponena za mmene anthu osakhulupilila anali kuonela Akristu a m’nthawi ya atumwi . ( 1 Akor . 8 : 8 ) Caciŵili , anawacenjeza kuti ‘ ufulu wawo ’ usakhale “ copunthwitsa kwa ofooka . ” ( 1 Akor . Ukadulidwa umaphukanso . ” Woyamba anati : “ Ngakhale kuti kugwila nchito ndi odzozedwa ndi mwai wapadela , kugwilizana kwambili ndi io , ngakhale kuti ndi odzozedwa ndi mzimu , kwandithandiza kudziŵa kuti abale amenewa ndi opanda ungwilo . Anthu acidwi akabwela ku misonkhano , amaona kuti ana athu amatengako mbali pa misonkhano . Ngati tikumbukila kuti tilibe mphamvu zoweluza ena , sitidzawasuliza kapena kukaikila zolinga zao . ( Luka 6 : 37 ; Yak . Mu 1945 , asilikali a ku Japan anacoka m’dziko lathu . Davide anakhumudwa na zimenezo . Kodi uganiza kuti n’cifukwa ciani anthu ni ankhanza conco ? ” 1 : 1 , 9 ) Ndithudi , cinali cilimbikitso cogwilia mtima ngako ! Msulamiyo anali monga “ khoma ” osati monga “ citseko ” cimene cimatseguka mosavuta . Ngati makolo asemphana maganizo pankhani ina , angacite bwino kukambilana mwamseli nkhaniyo ndi kumanga mfundo imodzi . KULANGA NDI KOFUNIKA 2 : 15 - 17 ) Ndipo tiyenela kukumbukila zimene zidzacitikila anthu ocimwa osalapa . 2 : 12 ) Mzimu wa dziko umalimbikitsa munthu ‘ kutsatila zilakolako za thupi lake . ’ Cifukwa coona khalidwe laubwenzi la mlongoyo komanso khama la Akhristu acikulilewo , kholo lina linavomela kuphunzila Baibo . ( 1 Akorinto 16 : 14 ) Ngati mumapatsa cifukwa ca cikondi ceniceni ndiponso cifukwa coganizila wolandilayo , iye adzalandila mphatso yanu mwacimwemwe , ndipo mudzakhala na cimwemwe cobwela cifukwa copatsa . M’bale wanga Jairo ali ndi umoyo wovuta ngati umenewo . Tonse mumpingo tingasonyeze kuti tili ndi cikondi ceniceni mwa kupewa kulankhulana ndi munthu wocotsedwa . Cotelo ngati mwakhumudwitsa munthu wina , muyenela kutsatila malangizo a m’Baibulo . Atumwi anathetsa vutolo mwamsanga mwa kuika amuna oyenelela mwauzimu kuti aziyang’anila nchito yogaŵila cakudya . Mwina kumene timakhala kulibe Mboni zambili kapena ndi anthu ocepa cabe amene amalabadila uthenga wathu . Malinga n’zimene dikishonale ina inakamba , umboni wakuti “ Ayuda anali kukonda kulumbila pa zilizonse , ” ni wakuti m’buku laciyuda lochedwa Talmud muli malangizo ambili ofotokoza malumbilo amene anali ololeka kuwasintha ndi amene sanali ololeka kuwasintha . — Theological Dictionary of the New Testament . Yesu analimbikitsa otsatila ake kuti : “ Khalani opatsa ndipo inunso anthu adzakupatsani . Dikishonale ina imati : “ Ndi munthu amene waona cocitika cinacake ndipo auzako ena cocitikaco . ” Kodi Mfumu Davide inafuna kucita ciani ? Nanga Yehova anati ciani ? Conco , uzikhala wokondwela ndi utumiki uliwonse , cifukwa utumikiwo ni wa Yehova . ” — 2 Akor . Mulungu “ akuletsa nkhondo mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ” 12 : 3 - 7 ) Kodi Mose anacita ciani ? Fotokozani zimene Nowa anayang’anizana nazo . Magulu aciwawa otunthiwa ndi ansembe anali kucotsa abale m’nyumba zawo na kuwacitila nkhanza zosiyana - siyana . ( Mateyu 26 : 52 ) Anthu amene analabadila uthengawo anakhala ndi cikondi colimba . Ndipo m’bale wa ku Canada amene tam’chula kuciyambi , anakamba kuti lomba amadziŵa kuti “ kaŵili - kaŵili , umbuli ni umene umayambitsa tsankho komanso kuti makhalidwe a anthu sadalila kumene anabadwila . ” Pamene n’nayamba kuphunzila Baibo , n’nali kuyelekezela zimene imakamba na zimene n’nali kuona pakati pa Mboni za Yehova . Ngakhale kuti Mulungu wawaitana kuti adzapite kumwamba , io adzalandila mphoto yao kokha ngati akhalabe okhulupilika . Yesu anali woyamba kuukitsidwa mwa njila yapadela imeneyi , ndiponso kuukitsidwa kwake kunali kofunika kwambili . Pamenepa , m’baleyu anaonetsa mzimu wodzimana , ndipo izi zathandiza kwambili abale na alongo osoŵa a m’delalo . Ndipo mofanana ndi anthu ena onse , Mboni za Yehova zimakumana na mavuto . NKHANI ZOSIYANA - SIYANA Kodi wacita zimenezi mwa njila yotani ? Pofuna kufotokoza kuti nkhani inayake ya m’Baibulo imaimila cinacake , kapolo wokhulupilika masiku ano amaonetsetsa kuti pali umboni womveka bwino wa m’Malemba . Posacedwapa , m’bwalo la Mfumu mudzakhala nyimbo za cisangalalo , ndipo makamu a kumwamba adzaimba mofuula kuti : “ Tamandani Ya , anthu inu , cifukwa Yehova Mulungu wathu , Wamphamvuyonse , wayamba kulamulila monga mfumu . Tsiku lina , munthu amene ndinali kugwila naye nchito anandiuza kuti ndingapeze mayankho a mafunso anga onse m’Baibulo . Conco , tinali kuyenda pa basi ndipo kenako pa galimoto yaing’ono kucoka mudzi wina kupita ku wina . Komabe , n’kofunika kuti ‘ tizimvetsela mwachelu kwambili . ’ Tikakumana ndi ciyeso , palinso zina zimene zimaloŵetsedwamo kuposa kuvutika kwathu . Pamene akulu athandiza okalamba monga kuwapezela cakudya kapena kuwakonzela nyumba , angacite bwino kutengako ena . “ Nchito zanu n’zazikulu ndi zodabwitsa , inu Yehova Mulungu , . . . Ifenso tiyenela kuganizila cikhalidwe ndi zikhulupililo za anthu a m’gawo lathu kuti tidziŵe nthawi yabwino yokamba nao . Mu January 1974 , ndinabatizidwa ndi kukhala wa Mboni za Yehova . M’gulu la Mulungu muli nchito zambili masiku ano . N’cifukwa ciani makolo ena amakhala na nkhawa pamene mwana wawo afuna kudzipeleka na kubatizika ? 15 : 23 - 26 ) Ndithudi , aja amene adzakhala padziko lapansi adzapindula kwamuyaya . Ni khalidwe liti la umunthu watsopano limene limatithandiza kwambili kukhala ogwilizana ? Mmodzi wa akuluakulu a asilikali ku United States atayendela kafiteliya yathu ku Yankee Stadium mumzinda wa New York , analimbikitsa Faulkner , mkulu wa Dipatimenti ya nkhondo ya dziko la Britain kuti nayenso akayendele kafiteliya yathu . Ngakhale n’conco , anapitiliza kutsatila zimene Wophunzila Baibulo wina dzina lake Konrad Mörtter anali kukhulupilila . Iye anati : “ Nazindikila bwino mfundo ya m’Mawu a Mulungu yakuti Mkhiristu sayenela kupha munthu . ” — Eks . Nkhani imeneyi itionetsa bwino cifukwa cake tiyenela kucita mwambo wokumbukila imfa ya Yesu . ( Genesis 2 : 8 ) Lonjezo la Yesu linapatsa munthuyo ciyembekezo cotsimikizika cakuti adzaukitsidwa m’Paladaiso pa dziko lapansi latsopano . Mfundo ni yakuti , mayankho amene angakhutilitse mwana wanu lelo , tsiku lina adzakhala osam’khutilitsanso . Kodi tingacite ciani kuti tikhalebe na “ mtendele wa Mulungu ” ? Mungacotse bwanji zopinga kuti muziimbila Yehova na mtima wonse ? Mukatelo wophunzila aliyense amene akufunitsitsa kuphunzila adzaona kuti mumam’konda ndipo adzakuyamikilani mocokela pansi pa mtima . Conco , tiyeni tikhale otsimikiza mtima ‘ kugwila mwamphamvu cimene cili cabwino . ’ Emil anali atatumizidwa ku ndende , ndipo kumeneko anakumana na Mboni . Koma zimenezo sizitanthauza kuti Mulungu amavomeleza makhalidwe oipa amenewo . — Ŵelengani Aroma 1 : 28 - 32 . Mwacitsanzo , Uthenga Wabwino wa Mateyu unali kudzaza mpukutu umodzi . Komanso nkhani za m’magazini ino kapena zopezeka pa webusaiti ya jw.org , pa cigawo cakuti “ Zimene Baibulo Limaphunzitsa , ” zingakuthandizeni kumvetsetsa tanthauzo la malemba ambili . Kodi nanunso n’zimene mumafuna ? Akopotala ( apainiya ) anagwila nchito yofunika kwambili yolalikila uthenga wa Ufumu ku nyumba ndi nyumba . Yesu anakhumudwa kwambili ndi anthu amene anali kucita malonda m’kacisi wa Mulungu ndipo anawapitikitsa . ( Yoh . Sebastian , wa zaka 21 , anati : “ Pamene niŵelenga Baibo , nimalemba vesi imodzi m’caputa iliyonse , na kuika pamodzi mavesi anga a pamtima . 16 , 17 . ( a ) Tikamakamba ndi acibale kapena anzathu , kodi tingatengele bwanji citsanzo ca Yesu ? Tsopano , kulibenso kuthamangathamanga kupita ku positi ofesi kukatumiza zinthu zimene zamasulilidwa . Ngakhale pamene amishonale anabwelako ku msonkhano wa maiko , n’napitiliza kutumikila pa Beteli . 3 : 14 , 15 ) Anthu angakhale a m’banja limodzi , koma makhalidwe ao ndi zokumana nazo pa umoyo wao zingakhale zosiyana . 45 : 16 - 20 . Koma Rakele anamwalila pamene anali kubeleka mwana waciŵiliyo . Nanga n’cifukwa ciani n’cosoŵa masiku ano ? Koma masiku ano , padziko lonse pali magalimoto oposa 1.5 biliyoni , ndipo m’maiko ambili muli miseu yabwino . Mwacitsanzo , Nsanja ya Olonda ya July 15 , 2008 inatithandiza kumvetsa bwino mafanizo a Yesu okhudza cofufumitsa , kambeu ka mpilu , ndi khoka . Atatsiliza maphunzilo , Riana anacitadi zimene analonjeza . Komabe , ena amacita manyazi kuimba pagulu . “ Sangalala mwa Yehova , ndipo adzakupatsa zokhumba za mtima wako . ” — SAL . Ndithudi , zimene Akristu amenewa amacita n’zolimbikitsa kwambili ! Kukhala ndi moyo wosatha m’mikhalidwe ya mtendele ndi yabwino popanda kudwala , nkhondo , njala kapena imfa , kudzacititsa kuti tikasangalale ndi madalitso kwamuyaya . Anamuuza kuti atenge ndodo yake , asonkhanitse anthu pafupi na thanthwe , na kukamba nalo thanthwelo kuti litulutse madzi . Awa ndi mau amene ali pa zikwangwani zikuluzikulu ku North America , ndipo akhalapo kwa zaka zoposa 100 . Caciŵili , tiyenela kucondelela Yehova m’pemphelo kuti atsegule mitima ya anthu oona mtima . ( Oweruza 10 : 7 , 8 ) Kuonjezela pa adani a Aisiraeli , Yefita anali kukumananso ndi mavuto ocokela kwa abale ake enieni komanso kwa atsogoleli a Aisiraeli . ( Salimo 102 : 25 , 26 ) Kelvin anakhulupilila zimene Baibo imaphunzitsa zakuti Mulungu angaletse kuti zolengedwa zake zisawonongeke . — Mlaliki 1 : 4 . Malemba amanena kuti ngakhale kuti Abulahamu ndi atumiki ena a Mulungu “ sanaone kukwanilitsidwa kwa malonjezowo ” m’nthawi yao , “ anawaona ali patali ndi kuwalandila . ” 62 : 7 , 8 ) Anafotokozelanso amene anali kum’phunzitsa Baibo , komanso ena mu mpingo . 1 : 3 ) Paulo anaonetsa kuti anali kuyamikila kukoma mtima kwakukulu kwa Yehova mwa kulalikila mwakhama . Kodi timatengela citsanzo cake ? — Ŵelengani Aroma 1 : 14 - 16 . Koma sanasunge lumbilo lake . N’nayamba kufuna kuphunzitsako ena coonadi . Anthu oona mtima amayamikila akadziŵa kuti Yehova , cifukwa ca cikondi ndi kukoma mtima kwake kwakukulu , anatuma Mwana wake padziko lapansi kuti adzatimasule ku ucimo ndi imfa . — 1 Yoh . Pali abale acinyamata amene amayang’anila nchito zimene zimaphatikizapo acikulile . Pa tsikulo , Arthur , anagona mocedwa cifukwa coganizila za mmene adzayendetsela motokayo . Cathy wa ku Britain , asanapite kudziko lina , coyamba anafufuza kuti adziŵe dziko limene lingakhale bwino kwa mlongo wosakwatiwa kukatumikilako . Izi zitanthauza kuti anthu analengewa na makhalidwe amene Mulungu ali nawo , monga cikondi na cilungamo . Anali atamenyedwa ndi mng’ono wake wazaka zinai , ” anatelo a NICOLE . Mwacitsanzo imati “ Mateyu wokhometsa msonkho , ” “ Simoni wina wofufuta zikopa , ” ndi “ Luka , dokotala wokondedwa . ” ( Mat . 10 : 3 ; Mac . 10 : 6 ; Akol . Pambuyo pake ndinapepesa cifukwa cocita zinthu mosawaganizila . Iwo anali ndi buku la Mungathe Kukhala ndi Moyo Kosatha limene anali kugwilitsa nchito pophunzila Baibulo mlungu uliwonse . Tikacita zonsezi tidzaonetsa kuti tikutsatila mau a mtumwi Paulo akuti , “ Mukufunika kupilila . ” Kumapeto kwa za 1000 , Satana adzaloledwa kuyesa anthu angwilo pa ciyeso cotsilizila . Kodi umaona kuti madalitso amene umapeza tsopano , ndi amene udzapeza mtsogolo ndi ambili kuposa mavuto amene ungakumane nao ? ” 1 : 3 ; Tito 1 : 5 ) Sitidziŵa ngati anafika ku Spain , koma anali ndi colinga copita kumeneko . — Aroma 15 : 24 , 28 . Iwo anazimanga ziŵili - ziŵili pa joko ndipo zonse zinali kulimila pamodzi m’mundawo . Baibo siikamba zambili pa nkhani imeneyi . Kodi udzakwanitsa bwanji kupeza zofunikila ukabwelela kunyumba ? ” Nkhaniyi idzafotokoza mmene tingaseŵenzetsele bwino mfundo za m’Baibo mu umoyo wathu . ( Onani kabokosi kakuti “ Zifukwa Zimene Ena Safunila Kugaŵila Ena Maudindo . ” ) Ŵelengani nkhani yotsatila kuti mudziŵe mayankho a mafunso amenewa . KUYAMBILA m’caka ca 1992 , Bungwe Lolamulila lakhala likusankha akulu okhwima kuuzimu , kuti azithandizila makomiti a bungweli kukwanilitsa nchito yao . Tiyenelanso kumapatula nthawi yophunzila nyimbozi kunyumba kwathu . Kucita izi kudzatithandiza kuti tiziimba na mtima wonse pamisonkhano . 4 : 31 . Iye anali kulambila Yehova , osati mulungu wina aliyense . 1 , 2 . ( a ) Kodi ciyembekezo ca Akhiristu oona cimasiyana bwanji na ciyembekezo ca anthu a m’dziko la Satana ? Sitiyenela kufulumila kumuweluza kapena kumukakamiza kusintha maganizo ake . A Yohane : N’zoona . 37 : 9 , 11 , 29 . Nili na zaka 14 , n’nali kuthela nthawi yambili kutolela mapepa kuti akapangidwenso kukhala atsopano pofuna kuteteza zacilengedwe . 1 : 2 ; 2 : 6 ) Zoona , Akhiristu a m’cikwati afunika ndithu kumaonetsanako cikondano cawo . Pogaŵa cakudya kwa akazi amasiye osauka , akazi amasiye okamba Cigiriki anali kunyalanyazidwa . ( Mac . Ayuda anali kucita zikondwelelo zitatu caka ciliconse ku Yerusalemu . Baibo ya Septuagint inathandizanso anthu mamiliyoni ambili amene sanali Ayuda ndipo anali kukamba Cigiriki , kudziŵa zimene Baibo imaphunzitsa . Kodi timabala bwanji zipatso ? Mafanizo ena amaphiphilitsila zinazake ndipo amakhala ulosi , koma ena amatsindika mfundo inayake yofunika . Koma bwanji ngati pofika mu mzindamo mupeza kuti mulibe malamulo a pamsewu . N’ciani cingatithandize kucepetsa nkhawa ? Wacicepele ameneyu anapindulanso ndi nkhani yakuti “ Kodi Mulungu Amavomeleza Makhalidwe a Kugonana Kwachilendo ? ” Iye anabwezela cuma conse cimene anapeza mwacinyengo , ndipo analeka kukhala na mtima wadyela . Kodi mumakhulupilila kuti “ mau awa ndi odalilika ndi oona ” ? Kulekelela anthu ocita macimo mwadala mumpingo kumasonkhezela ena kunyalanyaza miyezo ya Mulungu . Mauwa analembedwa m’zaka za m’ma 600 B.C.E . Imakamba Zoona pa Mbili Yakale : Zocitika zolembewa m’Baibo zigwilizana kwambili na mbili yakale yotsimikizika . Iwo anandilola kuti ndipite kunyumba . Ndipo imwe na iwo mudzalimbikitsidwa kupitiliza kuonetsa kuwala kwa coonadi . Kenako , anakamba mau osangalatsa akuti : “ Ali moyo tsopano . ” Anthu amene anaona zimenezi ayenela kuti analimbikitsiwa ngako . Pambuyo pokambilana ziyamikilo za abalewo ndi bungwe la akulu , woyang’anila dela ali ndi udindo woika akulu ndi atumiki othandiza mumpingo . Ndiyeno Birgit anawafotokozela kuti : “ Timaphunzitsa ana athu kutsatila mfundo za Mulungu za makhalidwe abwino , ndipo kucita zimenezi kumaphatikizapo kulemekeza atica . ” Nthawi zina , tinali kukangana cifukwa ca vuto la zacuma limenelo . ” Kumvetsela pamene akusimba za cisangalalo cimene ali naco kungalimbitse cikhulupililo ndi cidalilo canu mwa Yehova . Kodi ulamulilo wa Yehova tingaucilikize bwanji masiku ano ? Nkhani ino ifotokoza mmene kupezeka pamisonkhano ( 1 ) kumatipindulitsila , ( 2 ) kumapindulitsila ena , ndi ( 3 ) mmene kumakondweletsela Yehova . — Onani mau akumapeto . Panthawi yovuta imeneyo , Yehova ndi Mwana wake adzapulumutsa anthu amene amaitana pa dzina lake . ( 2 Akorinto 6 : 14 ) Koma pali abale ndi alongo ena amene ali m’banja ndi munthu amene si wa Mboni za Yehova . Cosangalatsa n’cakuti ambuya anabatizika pa msonkhano wacigawo ku Madrid mu August 2014 . ( Genesis 2 : 17 ) Koma munthu woyamba anapandukila ulamulilo wa Mulungu , ndipo anabweletsa imfa pa iye ndi ana ake . Makhalidwe amenewa ndi ofunika kwambili kuti banja likhale lopambana . Yesu anatumidwa kudzamasula anthu mu ukapolo wa ucimo na imfa . Popeza kuti anthu ambili amakamba kuti zinthu zonse zimene zimacitika ndi cifunilo ca Mulungu , ndinali kudzifunsa kuti : ‘ Kodi Mulungu amacititsa mavuto a anthu ndiyeno ndi kumakondwela akaona kuti akuvutika ? ’ M’masiku otsiliza ano , anthu alinso na makhalidwe ena oipa amene tiyenela kuwapewa . Baibo inakamba kuti anthu osaopa Mulungu adzakhala osakonda zabwino . ( 1 Akorinto 10 : 13 ) Baibo imatilonjeza kuti idzafika nthawi pamene mavuto athu adzatha , ndipo sadzakhalaponso ! Ifenso tifunika kulemekeza nyumba za ena . Masomphenya amene taŵelengawa , aonetsa kuti Yehova Mulungu , Yesu Khiristu , angelo okhulupilika , ndi anthu amene anagulidwa pa dziko lapansi , onse amatikonda ndi kutifunila zabwino . N’cifukwa ciani nimvela mwanjila imeneyi ? Ndiyeno sankhani Malemba amene angakuthandizeni kukwanilitsa zolinga zanuzo . Anali ndi ufulu wolambila , ndipo sanali kukakamizidwa kulambila milungu yaciroma . ( Yoswa 9 : 3 , 9 , 10 ) Ngakhale kuti mafumu ena anamva ndi kuona mmene Yehova anapulumutsila anthu ake , io “ anasonkhanitsa pamodzi magulu ao ankhondo kuti amenyane ndi Yoswa ndi Isiraeli . ” Kodi Yesu anaonetsa makhalidwe a Yehova m’njila ziti ? N’nakambilana ndi asilikali , ndipo mkulu wa asilikali wokoma mtima anatipatsa madzi akumwa panthawi yonse ya msonkhano . Anatumanso asilikali kuti adzatimangile matenti aŵili aakulu . Ina inakhala kicheni ndipo ina kafiteliya . Anaphunzila Baibulo ndi kuyamba kulalikila . Zimenezi zionetsa kuti iye amasamalila aliyense wa ife . Cimene Mulungu amafuna kwambili n’cakuti tidziŵe maganizo ake , mmene amamvelela , komanso malangizo amene amapatsa atumiki ake Ndithudi , Mulungu anamasula Aisiraeli mu ukapolo ku Iguputo , na kuŵapatsa ciyembekezo ca umoyo wamtendele ndi wacimwemwe m’Dziko Lolonjezedwa . ( Aroma 12 : 18 ) Kodi zimenezi n’zotheka ? M’Baibo , timaphunzila kuti Yehova amalamulila mwacikondi . ( Miyambo 18 : 1 ) Ngakhale kuti pali nthawi imene mungafune kukhala nokha , musakhale ndi cizolowezi codzipatula . “ Uthenga wabwino uwu wa ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” A Robert , amuna a Nicole , naonso amayesa kuona nkhani yonse . N’zoona kuti odzozedwa anazunzidwa panthawi ya nkhondo yoyamba . Koma amene anali kuwasautsa anali olamulila a dziko , osati Babulo Wamkulu . Mupite pa webusaiti yathu ya www.jw.org . Paulo atatsiliza kufotokoza kuti tifunika kuvala umunthu watsopano , anakambanso za kupanda tsankho , khalidwe limodzi mwa makhalidwe ofunika ngako a umunthu watsopano . Patapita nthawi , ana aŵili aakazi a M’bale Goslin analowa Sukulu ya Gileadi ndi kukhala amishonale . Kenako , Petulo anakana Yesu katatu . Panthawi ina , ophunzila a Afarisi ndi acipani ca Herode anafika kwa Yesu ndi kumufunsa pankhani ya msonkho . Melvin ndi Sharon a ku South Carolina , anagulitsa nyumba ndi katundu wao n’colinga cakuti akathandize panchito yomanga likulu ku Warwick . Pambuyo potumikila m’dela kwa nthawi yocepa cabe , n’naona kuti uphungu wake unali wofunikadi . ( Miy . 19 : 17 ; Mat . 6 : 3 , 4 ) Conco , tikathandiza anthu amene akuvutika , Yehova amaona zimenezo ngati nkhongole imene tamukongoza . Mwacibadwa ndinali wamtima wapacala , moti silinali vuto kukwiya msanga . Kodi anthu amene anadziŵa zoipa zimene Ahabu anacita , anamvela bwanji ataona kuti Mulungu wamucitila cifundo ? Anthu amaleka kukhulupilila boma limene limayesa kuthetsa cabe ziphuphu za apolisi ndi oyang’anila za oloŵa ndi otuluka m’dziko , koma amalekelela akuluakulu a boma amenenso amacita ziphuphu . ( Luka 22 : 28 ; Yoh . 14 : 12 ; 16 : 27 ) Tingadzifunse kuti , ‘ Kodi nimatengelako citsanzo ca Yesu mwa kuyamikila ana anga ndi ena pa zabwino zimene amacita , m’malo mongoyang’ana pa zimene amalakwitsa ? ’ Zikakhala conco , muyenela kupempha Yehova kuti akutsogoleleni ndi kukuthandizani kuti mudziŵe zimene mungacite . Tikamaonetsa cikondi , timapeza madalitso okhalitsa . 39 : 7 , 8 , 10 ) Malinga ndi katswili wina wa Baibulo , m’mau ena mkazi wa Potifara anali kunena kuti : “ ‘ Tiye ticezeko tili aŵiliŵili . ’ Popeza tili m’nthawi ya mapeto a dzikoli , tifunika kugwilitsitsa ciyembekezo cathu . Ataphunzila kuti dzina la Mulungu ni Yehova , anagwetsa misozi yacimwemwe . 2 Akorinto 12 : 9 , 10 Kuyambila kale , maboma alephela kusamalila anthu , makamaka osauka . 3 Kodi Angelo Amakhudza Umoyo Wanu ? Kenako anasankha kungonyalanyaza zimene zinacitikazo . Kodi padzakhala zotsatilapo zotani ngati mupitiliza kuphunzitsa ana anu acinyamata kuti azitumikila Yehova ? Ngati zimenezi zakucitikilani , kodi simungayamikile ngati wina angaonetse kuti amakudelani nkhawa ? Lemba la Chivumbulutso 11 : 3 limanena za mboni ziŵili zimene zinali kudzalosela kwa masiku 1,260 . Atumiki a nthawi zonse amene akutumikila ku dziko lina , ndipo ni oyenelela kuloŵa sukuluyi malinga na ziyenelezo , angafunsile kuti akaloŵe sukuluyi m’dziko lawo kapena ku dziko lina , kumene imacitikila m’citundu cawo . Nkhaniyi idzafotokoza zifukwa zake acicepele afunika kuika patsogolo nchito yolalikila , komanso kudziikila zolinga zauzimu akali aang’ono . N’naphunzila mfundo yofunika pamene n’nali kuthandizila M’bale Theodore Jaracz paulendo wina wokacezela nthambi . Koma kodi Mulungu wake , Yehova , anadziŵa mmene iye anali kumvelela ? Kucita mselu - selu . N’kuthekanso kuti anali kukamba zonse ziŵili . ( b ) Kodi mungam’thandize bwanji mwana wanu kuganizila madalitso amene angapeze cifukwa comvela malamulo a Mulungu ? Mungaŵelenge nkhani za abale ndi alongo amene Baibulo linawathandiza kusintha khalidwe lao . Kodi Khalidwe Lopambana n’ciani ? Ndipo tingalionetse motani ? Ngakhale kuti nthawi zina zimenezi sizingacitike kwa ife , tiyenela kutsatila citsanzo ca abale ndi alongo odzipeleka amenewa ndi kuika zinthu za Ufumu patsogolo . ( Yes . N’cifukwa ciani iye analengeza za kuukitsidwa kwa Kristu kwa atsogoleli acipembedzo amene anazonda Yesu ndi kucititsa kuti aphedwe ? Musatengele zocita za anthu amene sanaime zolimba ku mbali ya Yehova Kumbukilani kuti anangolakwitsa cabe ! Apanso , Yesu anatikumbutsa za cilengedwe ca Yehova . 20 : 1 - 7 ) Kodi Satana ndiye anacititsa zimenezo ? Ndi zinthu zotani zimene zinathandiza kuti uthenga wabwino ufalikile m’nthawi ya Atumwi ? Kwa kanthawi ndithu , Paulo sanali kufuna kuyenda ndi Yohane Maliko pa maulendo ao aumishonale cifukwa panthawi ina Maliko anasiya Paulo ndi anthu ena paulendo wao woyamba waumishonale . Tiyeni tikambilane zinthu zingapo zimene tingacite . Mulungu anauzila mtumwi Paulo kugogomeza mfundo yofunika kwambili imene ipezeka pa 2 Akorinto 6 : 4 . Izi zimafuna kukonzekela bwino . 1 : 1 ; Dan . 2 : 19 ) Ena analandila malangizo kupyolela mwa anthu oimilako Yehova , amene anali mbali ya gulu lake la padziko lapansi . Kodi maudindo tiyenela kuwaona bwanji m’gulu la Yehova ? ( Aroma 5 : 12 ) M’malo mopatsila moyo wangwilo kwa ana ake , Adamu anawapatsila ucimo umene unabweletsa imfa . Cimene cinam’thandiza kuleka ndi cimene cathandiza anthu mamiliyoni kumasuka kucizoloŵezi cokoka . Kodi cinthu cimeneco n’ciani ? Kodi mungacite ciani kuti muzigaŵa bwino nthawi yosamalila udindo wanu wakuthupi na wa kuuzimu ? Pewani Kutenga Mbali m’Ndale za Dziko Loipali , Apr . Munthu angandicite ciani ? ’ ’ — Aheb . Paulo anafotokoza mmene anthu adzayamba kucitila zinthu na anthu anzawo m’masiku otsiliza . Nanga Akhiristu akanawadziŵa bwanji anthu amene amamuimila ? Tifunika kukamba zinthu momveka bwino , koma tiyenela kupewa kukamba mwamwano kapena mopanda ulemu . — Ŵelengani 1 Akorinto 14 : 8 , 9 . N’zolakwa ziti zimene Yehosafati anacita ? Conco , ofesi ya nthambi inauza ofalitsa amene anali kudzakhala apainiya kuti m’dziko la Britain munalibe gawo lokwanila kutumikilamo , ndipo inawalimbikitsa kuti adzafunika kukacita upainiya ku maiko ena a ku Ulaya . ( 1 Petulo 4 : 4 ) Kodi Mkristu ayenela kubisa kuti ndi mtumiki wa Mulungu ? Sitingachule kuti ndi anthu angati amene anapenyelela “ Seŵelo la Eureka . ” 4 : 8 ; Yuda 20 , 21 . Ndi mwai wapadela kudzipeleka kwa Yehova ndi kubatizidwa . Ngakhale mumpingo wathu , muli zinthu zambili zimene tingacite potengela citsanzo ca amishonale . Blessing anati : “ Coonadi cimakumasula m’njila zodabwitsa . ” Mulungu safuna kuti wina aliyense akaonongeke . N’nali na mwayi wotumiza makope a buku lakuti The Finished Mystery a saizi ya m’thumba kwa abale ambili amene anali atalandidwa mabuku awo . Nanga mungacite ciani kuti imwe na munthu amene mwapatsa mphatso mukhale acimwemwe ? Ndipotu iye amatilimbikitsa kucita zimenezi . ( Miyambo 22 : 6 ; Akolose 3 : 21 ) Koma zimenezi sizitanthauza kuti zocita za banja lathu n’zimene zingaticititse kukhala munthu wabwino kapena woipa . Anasankha ndani ? Mtumiki wa Yehova Nowa anali kukhala m’dziko la anthu osaopa Mulungu , ndipo iye yekha na banja lake na amene anali kulambila Yehova . Erica anati : “ Poyamba ndinali kudzimva wotaika , koma zimenezo zinandithandiza kuganizila cimene ndinasamukila . Cikhulupililo ca Mose cinalimbikitsa anthu a Mulungu . Satana anakopa makolo athu oyamba Adamu na Hava , kuti akhale ku mbali yake popandukila Mulungu . Iwo angafote kapena kufa kumene ngati sathiliwa madzi . Koma angaphukile ngati asamalidwa bwino . Tsiku lina pamene anali kulalikila nyumba na nyumba , anakumana ndi mwamuna wina wavindevu . Ana angaonetse kuti amakonda makolo ao mwa kukamba nao pafoni nthawi zonse kapena kuwalembela makalata . — Miy . Kaya cifukwa cinali citi , Yohane analimbikitsa Gayo mwa kukamba kuti : “ Munthu amene amacita zabwino ndi wocokela kwa Mulungu . ” ( 3 Yoh . Ndipo palibe munthu woganiza bwino amene anafunika kukopeka ndi Baala ndi kuyamba kum’tumikila . Yehova amatiuza kuti tifunika kucita khama kuti titengele makhalidwe ake . Mtumwi Petulo analemba kuti : “ Cifukwa cakuti simukupitiliza kuthamanga nao limodzi m’cithaphwi ca makhalidwe oipa , anthu a m’dzikoli sakumvetsa , conco amakunyozani . ” ( 1 Pet . Nkhani ino itithandiza kuyankha mafunso amenewa , ndiponso ifotokoza mapindu amene tingapeze ngati tipeleka ulemu kwa amene ayenela kulandila ulemu . Kodi mudzapindula bwanji Mulungu akayankha pemphelo lanu lopempha mzimu woyela ? Anthu m’dzikoli sagwilizana pa zinthu zambili , ndipo ena amacita kumenyana cifukwa cosiyana maganizo . ( English as a Global Language ) Anthu ambili amaphunzila Cingelezi cimeneci , n’colinga cakuti acigwilitsile nchito pokambilana zamalonda , zandale , ndi zasayansi . Ngati panthawiyo acibale a Nowa anali ndi moyo , ndiye kuti naonso anaonongeka pa cigumula . ( Gen . Ngakhale n’conco , panali vuto lina . Kuwonjezela apo , Yehova amalamulila mwacikondi nthawi zonse . Malinga na Cilamulo ca Mose , agalu anali kuonedwa kuti ni nyama zodetsedwa . Mtengo akaunyula kuti auwokele pamalo ena umakwinyilila , koma akauwoka , umamela mizu yatsopano Nkhanizi zidzafotokoza nthawi imene anthu a Mulungu analoŵa mu ukapolo wa m’Babulo Wamkulu , ndi khama limene Akhiristu odzozedwa anaonetsa cakumapeto kwa ma 1800 kuti amvetse Mau a Yehova molongosoka . Anali atatengekeka ndi khalidwe lotamba zamalisece . Olo kuti anali kukonda mkazi wake kwambili , anali kugonjabe ku cizoloŵezi cimeneci nthawi ndi nthawi . Limapeleka malangizo oyenela a mmene gulu lifunika kuyendela pogwilitsila nchito mfundo za m’Baibulo . ( Onani cithunzi kuciyambi kwa nkhani ino . ) ( b ) Ni mafanizo othandiza ati amene mwaseŵenzetsapo ? Conco , kuti nkhaniyi tiimvetse bwino tifunika kupita ku Mau a Mulungu , Baibo . Popeza ndife Akhiristu , sitifunika kupepusa malangizo a Yesu akuti ‘ tikhalebe maso ’ m’masiku ano otsiliza . 3 : 1 ) Kodi tingatsimikize bwanji zimenezi ? ( Mac . 8 : 5 , 6 , 14 - 17 ) Conco , Asamaliya amenewo naonso anadzozedwa kukhala Isiraeli wa kuuzimu . Ngakhale kuti Yerusalemu anaonongedwa mu 70 C.E . , gulu limenelo silinaonongedwe . Akuluwo analimbikitsa mwamuna kuti ayenela kutengela citsanzo ca Yesu . M’malomwake , tinamuyandikila kwambili , pokhulupilila kuti adzakonza zinthu m’njila yoyenela komanso pa nthawi yake yoyenela . Cikondi sicitha . ” — 1 Akorinto 13 : 4 - 8 . Cimwemwe : Mukadziikila zolinga na kuzikwanilitsa mumamvela bwino mu mtima podziŵa kuti mwacita zimene munali kufuna . Makolo ayenela kulanga ana ao mwacikondi . Ndipo ayenela kupewa kuwalanga pamene ali okwiya . Yehova ayenela kukhala patsogolo mu umoyo wathu . 9 ( Yakobo 3 : 6 ) “ Lilime ” likutanthauza luso lathu lokamba zinthu . Baibo imalangizanso mwamuna kuti azikonda mkazi wake . Kodi pambuyo pake munazindikila kuti zinthu zimenezo zinali zosafunikila kwenikweni ? M’dzikoli , anthu ena ali na udindo wolamulila . Mbili ya Mlongo Padgett inalembewa mu Nsanja ya Olonda ya October 1 , 1995 masa . 19 - 24 . Iwo anamva cisoni kwambili . ( b ) kudziikila zolinga zabwino ? Pa cifukwa cimeneci , kudzikonza kwathu ndi zovala zimene timasankha , siziyenela kukondweletsa ife cabe . Nthawi zina kunali kubwela anthu ambili , ndipo anali kufunsa mafunso ambili mpaka usiku . Apanso pali phunzilo labwino limene tingatengepo kwa Rehobowamu . Iye moleza mtima ndi mwacikondi , amayandikila anthu opanda ungwilo . Mzimayi wina wodziŵika wa ku Sunemu waciisiraeli , anaceleza Elisa mwacikondi kwambili . Mu 1960 , nditatsiliza maphunzilo anga a m’hotelo , ndinabwelela kwathu kuti ndikathandizile acibale anga kuphunzila coonadi . M’bale wina ku Australia analemba kuti : “ Palibe nchito yovuta monga kuthandiza ana ako kukhala na cikhulupililo . Mwina fanizo lingathandize kholo kuona kuti si kwanzelu kukhulupilila zimenezi . ( b ) Kodi kusakhala pamodzi monga banja kungakhudze bwanji cikondi ndi khalidwe la banja ? Tingatsimikize bwanji kuti tikumvetsa zimene mafanizo a Yesu amatanthauza ? Mtundu udzaukilana ndi mtundu wina , ndipo ufumu udzaukilana ndi ufumu wina . ” Panthawi yake , Mulungu anapatsa Abulahamu mwana monga mmene anam’lonjezela . — Gen . Kodi anakhala na maganizo amenewa cifukwa ca malangizo oipa amene anthu ena anam’patsa ? Kodi mauthenga osoceletsa ndi oopsa bwanji ? Amuna okwela pa mahosi abweletsa mavuto padziko lapansi . Koma kumvetsetsa nkhani yake , kungakuthandizeni imwe na banja lanu kukhala na ciyembekezo ca tsogolo labwino . Kodi Baibulo Likusinthabe Umoyo Wanu ? Komanso zinawononga ubale wake ndi Mlengi . — Gen . Mulimonsemo , cifukwa ca kudzikuza , Hezekiya “ sanabwezele zabwino zimene anacitilidwa . ” 25 : 14 ) Conco , matalente amaimila nchito yolalikila ndi kupanga ophunzila . Mwacidziŵikile , iye adzakopa anthu mwa kuwalimbikitsa kukhala na mtima wadyela , ngati mmene wakhala akucitila nthawi yonseyi . Conco , Akristu onse okhwima kuuzimu kuphatikizapo akulu , ayenela kuthandiza abale acicepele ndi acatsopano kupita patsogolo . Komabe , zingakhale bwino kuti ana azipezeka pa misonkhano ya citundu cimene amamvetsetsa cifukwa amaphunzila zambili , mwinanso kuposa mmene makolo angaganizile . Panthawiyo , iwo anali na zaka 56 , ndipo amayi anali na zaka 35 . ( 1 Maf . 19 : 19 - 21 ; Neh . 7 : 2 ; 13 : 13 ; Mac . ( b ) Kodi kalata imene Paulo analembela Akhristu a ku Tesalonika ionetsa kuti ni nchito yanji imene inamupatsa cimwemwe ceni - ceni ? Pomaliza pake , mkaziyo “ anam’gwila malaya mnyamatayo n’kumuuza kuti : ‘ Ugone nane basi ! ’ ” Izi zinacitikanso m’nthawi ya atumwi . Kapena linali tsiku limene munabatizidwa ? Zioneka kuti anavutika kwambili ndi matendawo . Timakondwela kucita zinthu zofunika zimenezi , ndipo sitiona kuti n’zovuta kapena zolemetsa . Kodi Mau a Mulungu angatithandize bwanji ngati tili na nkhawa kwambili cifukwa ca mavuto ? 2 : 9 ) Ali kumeneko ca m’ma 62 C.E . , ndi pamene anauzilidwa kulemba kalata yake yoyamba . Sitiyopa kucita nchito zabwino mu utumiki wa Yehova poganiza kuti Satana adzationa . Kodi Cilamulo cinatumikila mbali iti maka - maka ? Nkhani yaciŵili idzafotokoza makhalidwe angapo amene ali mbali ya umunthu watsopano . Nthawi zina , banja lonse linali kusonkhana pamodzi kuti limvetsele nkhaniyo . Aisiraeli analibe ufulu woyenda cifukwa coopa adani awo . 19 , 20 . ( a ) Ni madalitso anji amene timapeza tikalandila cilango ca Mulungu ? Maganizo amenewo ofuna kucilikiza kulambila koona , ni amenenso anali na Yakobo mwana wa Isake , amene ana ake anadzakhala makolo a mafuko 12 a Israeli . Cifukwa zida zimenezi zifotokoza mfundo za m’Baibo zimene zathandiza anthu ambili kulimbitsa vikwati vawo . Ngakhale pamene colinga ndico kuthandiza winawake , kukambitsilana kwa conco n’kosafunika malinga n’zimene tangokambitsilana . Iye amakulitsa makhalidwe amenewa kuti apindulitse ena , osati ndi colinga cakuti ayenelele udindo . Izi zimacitika cifukwa cakuti thupi limapeleka magazi ku ziwalo zofunika kwambili . Olo kuti zinthu zingatiyendele bwino cifukwa cokana kuvomeleza colakwa cathu , tifunika kukumbukila kuti pothela pake , “ aliyense wa ife adzadziŵelengela mlandu wake kwa Mulungu . ” — Aroma 14 : 12 . Masiku ano , anthu ambili amapondeleza ofooka kuti apeze zimene akufuna . Kwazaka zambili anali woyanganila Service Department . Koma sikuti anthu onse amene timakumana nawo ni aukali . 24 : 15 . Kodi mtumwi Yohane akutithandiza bwanji kumvetsetsa kufunika koonetsa cikhulupililo ? Pomanga mfundo imodzi pankhani ya zikhulupililo kapena popeleka malangizo ku gulu , akulu odzozedwa ndi mzimu amenewo anali kutsogoleledwa ndi Malemba . — Mac . 1 : 20 - 22 ; 15 : 15 - 20 . Anafotokozela Toñi kuti anali na mavuto ake komanso a m’banja . Mwina mukhoza kumaganizila zinthu zina uku mukuŵelenga . Phili loyamba liimila ulamulilo wa Yehova wosatha komanso wa cilengedwe conse . Cinanso , kudzipeleka na mtima wonse kutumikila m’dela lathu kapena kukatumikila ku dziko lina , kumatithandiza kukonzekela mautumiki osiyana - siyana a m’dziko latsopano . Kunena zoona , mabungwe acinyengo amenewa ndiwo acititsa mavuto ambili amene asautsa anthu padzikoli . Iwo anamuuza kuti : “ Khulupilila mwa Ambuye Yesu ndipo udzapulumuka . ” — Mac . 16 : 25 - 34 . Mmene Yesu anali kucitila zinthu paumoyo wake zinaonetsa kuti iye anali wozindikila . Tiyenelanso kuyesetsa kuthandiza ena mwauzimu . Amapewa kugwilizana ndi anthu amene amacita zosalungama . Mu 1989 , ndinali ndi mwai wopita ku Romania ndi M’bale Theodore Jaracz , wa m’Bungwe Lolamulila . Baibo imati ‘ Mulungu anatisonyeza ife cikondi cake mwa kutumiza Mwana wake wobadwa yekha . ’ Nikumasulila nkhani ya M’bale Albert Schroeder Usalile . ” N’zoona kuti tonsefe tili ndi zofooka zinazake ndipo nthawi zina timakhumudwitsa ena . Ndinakulila ku Los Angeles , mu mzinda wa California , ku U.S.A , kumene ciwawa ndi mankhwala osokoneza bongo n’zofala . Ngakhale kuti anali wokongola kwambili cakuti anakopa mfumu imene panthawiyo inali ndi “ mafumukazi 60 , adzakazi 80 ndi atsikana osaŵelengeka , ” Msulami anali kudziona ngati “ duwa lonyozeka la m’cigwa ca m’mphepete mwa nyanja . ” M’zaka za m’ma 1940 , anthu anacita kafuku - fuku pa nkhani ya kudziletsa , koma kafuku - fuku waposacedwa waonetsa kuti masiku ano , vuto la kusadziletsa kwa anthu lafika poipa kwambili . Pomasulila kucokela ku Cigiriki coyambilila , Hutter anaseŵenzetsa dzina lakuti “ Yehova ” ( יהוה , JHVH ) pa maina audindo akuti Kyʹri·os ( Ambuye ) , ndi The·osʹ ( Mulungu ) . Anali kucita izi pa mavesi aliwonse ogwila mau Malemba a Ciheberi , kapena akaona kuti vesilo ikukamba za Yehova . Izi zinacitika pamene atumwi onse anafa . Ndi nthawi pamene timaika pambali nkhawa za tsiku ndi tsiku ndi kuika maganizo athu pa za kuuzimu . Zimenezo zinandidabwitsa kwambili . Adamu na Hava anataya moyo umenewu . — Chivumbulutso 21 : 3 - 5 . Mboni za Yehova zingakonde kukuonetsani mmene zimaphunzilila Baibulo ndi anthu kwaulele , ndipo phunziloli limakhala la mphindi 10 kapena kuposelapo mlungu uliwonse . Mkristu wofikapo kuuzimu amakonda malangizo a Yehova . Nanga n’ciani cinam’thandiza kuyambanso kuona zinthu moyenela ? ( Neh . 7 : 2 ; 13 : 12 , 13 ) Olo masiku ano , “ cofunika kwa woyang’anila ndico kukhala wokhulupilika . ” ( 1 Akor . Popeza dziko limene tikukhalamoli n’loipa , kodi tingacite ciani kuti tikhale “ tiana pa zoipa ” koma “ aakulu msinkhu ” pa “ luntha la kuzindikila ? ” — 1 Akor . Cifukwa cakuti Yehova waika kale Yesu Kristu kukhala Wolamulila , ndipo iye amakonda anthu komanso ndi woyenelela . Angawafunsenso ngati anaphunzilako pamodzi kabuku kakuti N’zotheka Banja Lanu Kukhala Lacimwemwe . ( Zek . 2 : 8 ) Monga mmene mayi amakondela mwana wake , Yehova nayenso amathandiza anthu ake mwacikondi . Ngakhale abale athu ena sakudya mokwanila . Kutsatila mfundo za m’Baibo kumathandiza munthu kusintha khalidwe lake ( Onani palagilafu 16 ) Akulu ena amayendela akaidi m’ndende kuti akawaphunzitse Baibo kapena kukacititsa misonkhano . Sitifuna kukhala monga Diotirefe , amene sanalandile abale amene anacezela mpingo wake cifukwa cakuti sanali kuwalemekeza . Ganizilani mmene munthu anapangidwila . Conco amene ali ndi akazi azikhala ngati alibe , . . . Amene amagwilitsila nchito dzikoli azikhala ngati amene sakuligwilitsila nchito mokwanila . ” ( 1 Akor . 14 : 29 ; 15 : 28 ; 19 : 2 . Timacita zonse zimene tingathe kuti tithandize wophunzila Baibulo , koma sitiyenela kuiwala kuti munthuyo ayenela kusankha yekha kuti adzipeleke . Yesu anati : “ Zimene ndikuuza inuzi ndikuuza onse , Khalani maso . ” Mwina iyai . 12 : 13 ) Danieli wokalambayo anadziŵa kuti akufa akupumula ; ali ku manda , kumene kulibe ‘ kuganiza zocita , kudziŵa zinthu , kapena nzelu . ’ Mofanana ndi Asa , inunso mungaonetse kuti muli ndi mtima wathunthu mwa kudalila Mulungu na mtima wonse ngakhale pamene mukumana ndi citsutso cooneka ngati cosapililika . Conco , Paulo anawafunsa kuti : “ Bwanji osangolola kulakwilidwa ? ” ( 1 Akor . Adzacotsanso “ mpweya ” woipa wa m’dzikoli kapena kuti cisonkhezelo coipa ca Satana ndi ziwanda zake . — Aef . Opanga ngalawa akale anali kugwilitsila nchito mtundu wamadzimadzi . Tidzaphunzilanso cifukwa cake Mboni zimakhulupilila kuti zili ndi coonadi . Komabe , pali gulu la amuna ooneka ndi maso , amene ndi “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” Kapoloyu ndiye atsogolela anthu a Mulungu masiku ano . ( Mat . 13 , 14 . ( a ) Tiyenela kukumbukila ciani ponena za oyang’anila dela ? M’malo moleka kundipatsa mwai wopemphela , iye nthawi zonse anali kundiuza kuti ndipemphele pa kukumana kokonzekela ulaliki . Koma patapita nthawi , akulu - akulu a machechi anapanga colakwa cacikulu . Mau amenewa amam’kumbutsa Rose kuti ngakhale ali na matenda , Mulungu amasangalala na zimene amacita cifukwa ndiye zimene angakwanitse . M’maiko ambili , kodi ana aakazi amaonedwa bwanji ? Mwacitsanzo , ena akudwala matenda aakulu . Pamene zinthuzi zikucitika , Iye wapitilizabe kucititsa kuti cifuno cake cikwanilitsidwe mosasamala kanthu ndi zimene wotsutsa aliyense , monga Satana , angacite kuti alepheletse kukwanilitsidwa kwa cifunilo ca Mulungu . Monga wacicepele , kodi ungathandize bwanji anthu mogwila mtima pokambilana nawo za cilengedwe na za Baibulo ? Anthu amakamba kuti ndimadziŵika ndi kumwetulila kwanga . Mkristu ayenela kupewa kuyamba cisumbali ndi wosakhulupilila ( Onani ndime 14 ) Iye anali kulipila kudzela mwa oweluza . ’ Kunena kwina tingati , oweluza m’khoti anali kuuza wovulaza mkaziyo kuti alipile faindi kwa mwamuna wa mai wovulazidwayo . Mu mpingo wathu wa ku Tokmok , tinakhala na mwayi wocitako mautumiki ena . Anapitilizabe kuyenda na Mulungu . Ndipo ine ndikum’peleka kwa Yehova . Mwacitsanzo , kutsatila uphungu wakuti tizikhala okhulupilika kwa mnzathu wa m’cikwati kwathandiza cikwati cathu kukhalabe colimba . — Aheberi 13 : 4 . Motelo , Akristu oona , amene ali ndi cikumbumtima cophunzitsidwa Baibulo , saphunzila nkhondo kapena kutengako mbali m’nkhondo . Ndingakonde kukuonetsa dzinalo m’Baibulo . ” ▪ “ Limbani m’Cikhulupililo ” Panthawi ya mavuto imeneyo , tidzafunika kukhala ogwilizana kwambili . Mosakayikila , Paulo anaimvetsetsa kwambili mfundo imeneyi . Umboni wa zimenezi ni mau amene iye analembela abale a ku Filipi ofotokoza za nkhawa na mtendele wa Mulungu . Mwacionekele , Yehova ndiye anacititsa kuti Davide amenye Goliyati kamodzi - n’kamodzi . Ciwonjezeko cimeneci cimafunanso kupulintha mabuku ambili ophunzilila Baibo , kumanga ndi kukonzanso Nyumba za Ufumu , ndi mabwalo a misonkhano ya dela ndi ya cigawo . Dziŵani kuti cikwati si mpikisano wodziŵila kuti wolimba ndani , wodziŵa kunyoza mofuula ndani , kapena wodziŵa kulankhula mokhadzula ndani . Kapena tingakhale na nkhawa kwambili ndi mavuto amene tikumana nawo cakuti tingalephele kuika maganizo athu pa nkhani yaikulu imeneyi . Kodi Elihu anakamba ciani ponena za utumiki umene timacita kwa Yehova ? Conco , tikacita chimo , timavutika mumtima . Akhristu ena amene anacita chimo lalikulu afika poona ngati kuti Mulungu sangawakhululukile . Koma kodi kucita zimenezo ni nzelu zopindulitsa ? N’cifukwa ciani Paulo anacitila cifundo ofooka ? Mwina munthuyo amakhulupilila zimenezi cifukwa amafuna kuti anthu oipa akalandile cilango cifukwa ca zoipa zimene anacita . 29 : 25 . Ndipo izi zimacititsa munthu kukhala na mwayi wokhala paubwenzi na Yehova kwamuyaya . Tidzapitilizabe kupempha kuti cifunilo ca Mulungu cicitike mpaka Ufumu wa Mulungu utacotsa adani ake padziko lapansi . Iye adzaona kuti mumam’konda , ndipo adzakulemekezani kwambili . Sitiyenela kukayikila kuti “ munthu wopatsa mowoloŵa manja adzalandila mphoto . ” Pokhala atumiki a nthawi zonse , ise apainiya apadela tinali kuyembekezela kuti boma lidzatipatsa ufulu wakuti tisamagwileko nchito yocilikiza nkhondo , molingana ndi atumiki a machechi ena . Nkhawa Zokhudza Ngozi 8 Mwanjila imeneyi , timatsatila malangizo a Yesu okhudza ulaliki , amene ali pa Mateyu 10 : 11 - 13 , akuti “ Pamene mukuloŵa m’nyumba , pelekani moni kwa a m’banja limenelo . Ndipo kuleza mtima n’kofunika kwa Akhristu onse . Baibulo limanena kuti anthu a m’madela amenewa anali kukangana . ( Yoh . M’malomwake , zimaimila zinthu zonse zimene Yehova ndi Yesu adzacita mtsogolo kuti tidzakhale ndi moyo wosatha . — Yesaya 35 : 5 , 6 . Franz . Pambuyo pa zaka zingapo , n’naitanidwa ku ofesi ya M’bale Nathan Knorr , amene anali kutsogolela nchito ya padziko lonse panthawiyo . Mlongo Heidi wa zaka za m’ma 80 , sakwanitsa kulalikila kunyumba ndi nyumba monga mmene anali kucitila kale . ( Aroma 12 : 6 - 8 ) Popeza kuti Yehova wationetsa kukoma mtima kwakukulu , tili ndi udindo wogwila nchito mwakhama mu ulaliki , wophunzitsa ena Baibulo , wolimbikitsa abale ndi alongo athu , ndi kukhululukila aliyense amene watilakwila . Iwo amati akututa zimene anacita m’miyoyo ina asanabadwenso . ” Pa webusaiti imeneyi pali zofalitsa zofotokoza uthengawu m’zinenelo zoposa 700 . ( Oweruza 4 : 10 ) N’zosakaikitsa kuti asilikali analimbikitsidwa kwambili , kuona kuti mkazi wolimba mtima ameneyu akupita nao kunkhondo . Iye anaika moyo wake pangozi cifukwa ca cikhulupililo cake mwa Yehova Mulungu . Mulungu amawaona kuti alibe ucimo monga mmene amaonela Mwana wake Yesu , amene ndi wangwilo . 38 : 10 - 12 ) Zimenezi zikadzacitika , mwamsanga Yehova adzacitapo kanthu mwa kuukila Gogi ndi anthu ake . [ 1 ] ( ndime 14 ) Zofalitsa zimenezo ziphatikizapo buku la Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa , Buku Loyamba ndi Laciŵili , ndiponso nkhani zakuti “ Zimene Achinyamata Amafunsa , ” zimene zimapezeka pa intaneti . ( b ) Ndi zinthu ziti zimene mukuyembekezela m’dziko latsopano ? Koma zoona n’zakuti akungokatenga cabe mankhwala kapena kukalipila ndalama cabe kwa dokota . Mwacionekele , io anali kufuna kuti mwana wao akhale ndi tsogolo losiyana kwambili ndi zimene mwanayo anasankha . Mwana wa Mulungu wakhala akuonetsa kuti ndi wodzicepetsa kuyambila ali kumwamba monga colengedwa cauzimu , ndiponso panthawi imene anali padziko lapansi monga munthu wangwilo . Kodi Yehova amatitonthoza bwanji tikakumana ndi mavuto ? Nanga Mau ake amatitsimikizila ciani ? ( Yoh . 13 : 35 ) Kuti tipambane polimbana ndi Satana , tifunika kupewelatu kunyada kwa mtundu uliwonse . — Miy . Mlongosi wake , Esther , anati : “ Ngati ana amakamba citundu ca makolo , amayambanso kukonda cikhalidwe ndi cipembedzo ca makolowo . ” Mu vesi 1 , masiku a ukalamba amachedwa “ masiku oipa . ” Pa nthawiyo , azikulu anga 4 anali atacoka kale pa nyumba n’kukayamba nchito ya uphunzitsi . Ni madalitso ati amene timalandila kwa Yehova ? Cifukwa imaonetsa kuti Yehova anatilenga ndi ufulu wosankha zocita , kapena kuti nzelu za kuganiza ndi kusankha zocita . Zikuoneka kuti m’nthawi ya atumwi , Akristu onse oona anali odzozedwa . Mungamuyankhe bwanji munthu amene amakamba kuti kulibe Mlengi ? Iye analoŵa m’khamu la anthu , kudzela kumbuyo kwa Yesu ndi kumugwila malaya . Iye akumbukila kuti panthawiyo anamvela cisoni kwambili . Kucita zimenezi kunalimbitsa ubwenzi wanga ndi Yehova . Mofananamo , pali zinthu zambili zimene sitingathe kuzilamulila pamene tiyembekezela kukwanilitsidwa kwa malonjezo a Yehova . ( Maliko 13 : 32 , 33 ; Mac . Limapenda mosamalitsa ziyeneletso za m’Malemba za abale amene asankhidwa kuti aikidwe pa udindo mumpingo . Iye anayamba kulalikila kwa acibululu ake onse . Ngati mabungwe ofalitsa nkhani kapena amtolankhani akukamba mokondela , tifunika kukhala osamala kuti tisatengele maganizo ao . 8 , 9 . ( a ) N’cifukwa cina citi cimene timagwilila nchito yolalikila ? Tsopano , ndimapanga sopo yochapila ndi yosambila . 5 : 22 ; 6 : 1 ) Kodi timacita bwanji tikafika pa malile amenewo ? N’ciani cingatithandize kuti kusamalila okalamba kusakhale kotopetsa ? Uphungu umene Yehova anapatsa Yobu unam’thandiza ngakhale pamene mavuto ake anatha . Iye anali Hilda . Kodi mfundo ya m’lamulo limeneli itiphunzitsa ciani ? Amakhala alibe mtendele wa m’maganizo cifukwa codziŵa kuti cinthu coyenela kucita ni kukhululuka Anthu mamiliyoni padziko lonse amakhulupilila kuti Khrisimasi ni mwambo wokondwelela tsiku la kubadwa kwa Yesu Khristu . Mwacitsanzo , ngati ndinu kholo , mungauze ana anu zimene mumayamikila pa kupita kwawo patsogolo kuuzimu . Mofanana ndi Mose , sitiyenela kuika maganizo athu pa zinthu zooneka ndi maso . Iye atakwanitsa miyezi itatu , amai ake anam’bisa pakati pa mabango a mumtsinje wa Nailo , mmene mwana wamkazi wa Farao anam’peza . M’kupita kwa nthawi , khalidwe lathu labwino lingathandize anthu ena kusintha maganizo awo olakwika ponena za Mboni za Yehova . Banja lina la ku Rwanda limene lili ndi ana acinyamata anai , linasangalala kwambili pamene Baibulo la Dziko Latsopano linatulutsidwa m’cinenelo cao . Ni maudindo ati amene atumwi ndi akulu ena ku Yerusalemu anali nawo m’zaka 100 zoyambilila ? Kodi nimayesetsa kusakila mipata yodzidziŵikitsa kuti ndine wa Mboni za Yehova ? ’ Kaya mwakhala m’banja kwa nthawi yaitali kapena ai , muziganizila zimene mungakambe ndi kucita kuti mulimbitse banja lanu . Ngakhale zinali conco , Yehova kupitila mwa mneneli wamkazi Debora , analamula Baraki kuti : “ Tenga amuna 10,000 pakati pa ana a Nafitali ndi ana a Zebuloni ndipo mukasonkhane paphili la Tabori . Ulaliki Wapoyela ndi njila yothandiza imene timagwilitsila nchito kuti tifikile anthu ambili masiku ano . ( Ŵelengani Ekisodo 19 : 5 , 6 . ) Mkazi wa Hiberi , Yaeli ndi amene analipo . Kodi kuphunzila ndi kugwilitsila nchito Mau a Mulungu kumatithandiza bwanji ? N’ciani cinathandiza Yeremiya kukonda coonadi ca m’Malemba ? N’cimodzimodzi ndi ife asilikali a kuuzimu a Yehova . Kodi Yobu anadziŵa bwanji coonadi ponena za Mulungu ? Mwacitsanzo , iye amatengela Yesu ndi kukhala ndi umunthu watsopano umene “ unalengedwa mogwilizana ndi cifunilo ca Mulungu ndipo umatsatila zofunika pa cilungamo ceniceni ndi pa kukhulupilika . ” 9 “ Mulole Kuti Kupilila Kumalize Kugwila Nchito Yake ” Pa cocitika ciliconse , tidzaona mfundo ya m’Baibo imene ingatithandize kupanga cosankha mwanzelu . Mungaganizilenso zitsanzo zina za m’Baibulo . Davide ali mwana anadzozedwa ndi Yehova kuti adzakhale Mfumu ya Isiraeli m’tsogolo . Koma atsogoleli acipembedzo aciyuda onyada anacititsidwabe khungu ndi Satana komanso cifukwa ca mzimu wao wonyada . M’bale Mumba : Zoona n’zakuti Mboni za Yehova zimam’khulupilila Yesu . N’cifukwa ciani mufunika kuphunzila kugwilitsila nchito “ luntha la kuganiza ” mukali acinyamata ? Zimenezi zitanthauza kuti tifunika kucitapo kanthu kuti tilandile mphatso ya moyo wosatha . Mosamalitsa ndiponso mwapemphelo , amapenda ziyamikilo zocokela kwa akulu , ndi kuika pa udindo abale amene akwanilitsa ziyeneletso . Makolo anu anadya mana m’cipululu koma anamwalilabe . 1 : 8 ) Yehova anatanthauza kuti makolo onse aŵili afunika kukhala pamodzi kuti azilangiza ndi kuphunzitsa ana ao . Mu 538 kapena mu 537 B.C.E . , Koresi analamula Ayuda kuti abwelele kwao kukamanganso kacisi wa Mulungu ku Yerusalemu . Mwa kucita zimenezi , iye anapatsa mbadwa za banja loyamba mwai wosangalala ndi moyo wangwilo wofanana ndi umene Adamu ndi Hava anali nao . Sinikayikila ngakhale pang’ono kuti Yehova akatipatsa utumiki , amatipatsanso ciliconse cofunikila . Yesu ataphedwa , ansembe aakulu ndi Afarisi anapita kwa Pilato ndi kunena kuti : “ Bwana , ife takumbukila kuti wonyenga uja adakali moyo ananena kuti , ‘ Patapita masiku atatu ndidzauka . ’ Anali kufuna kunithandiza kuti nikonzenso ubwenzi wanga na Mulungu ndipo sananisiye . POYAMBA Satana anali mngelo wabwino wa Yehova . Buku lomaliza limatiuza za nthawi imene imfa idzaonongedwa ndi kuti Mulungu adzabwezeletsa Paladaiso padziko . 11 : 9 . ( Luka 11 : 4 ) Conco , ngati tikhululukila ena , ndiye kuti timakhulupilila Yehova . ( Mateyu 13 : ​ 18 , 19 ) Pokonza nthaka , mlimi amagwilitsila nchito zida zosiyanasiyana . Njila imodzi ndi kuŵelenga Mau a Mulungu . Naonso okwatilana ayenela kucitilana zinthu zimene angafune kuti azicitilidwa . Kulolelana m’cikondi kumaphatikizapo zambili . Komabe , tingathetse mavuto amenewa kapena kuwapewa mwa kutsatila uphungu wa m’Mau a Mulungu , Baibo . NYIMBO : 52 , 65 Mu May 1927 , Ophunzila Baibulo okangalika analalikila poyela kuti aitanile anthu ku nkhani za m’Baibulo . Kulemela si umboni wakuti Mulungu watidalitsa . Koma kukopana , kapena kulola kuti wina atikope , kungayambitse maganizo oipa amene angatipangitse kucita ciwelewele . Mu 1473 , Khiristu asanabwele , mtunduwo unali m’dziko la Mowabu , ndipo unali wokonzeka kuoloka Mtsinje wa Yorodano ndi kulanda Dziko Lolonjezedwa . ( Aheb . 11 : 8 , 13 , 15 , 16 ) Mose anafulatila cuma ca Aiguputo , “ ndipo anasankha kuzunzidwa pamodzi ndi anthu a Mulungu , m’malo mocita zinthu zosangalatsa koma zosakhalitsa zaucimo . ” ( Aheb . Sachio anawonjezela kuti : “ Tinaganiza zopita ku Yangon , mzinda waukulu ku Myanmar n’kukakhalako kwa wiki imodzi . Naphunzila kudalila Yehova na gulu lake , ndipo napindula ngako cifukwa cocita zimenezo . Tiyeni tikambilane citsanzo ici : Yelekezani kuti mnzanu wakupatsani galimoto . Iye anatiphunzitsa zinthu zina zocepa zothandiza poyendetsa boti . Anatiuza mokwezela ndi kutsitsa nsalu za boti , moseŵenzetsela kampasi , ndi motetezela boti kumphepo ya panyanja . Acibululu a Naboti na mabwenzi ake anali ndi cisoni cacikulu kaamba ka zinthu zopanda cilungamo zimene Ahabu anacita . Ndipo mosakayikila , iwo anatonthozedwa atazindikila kuti Yehova anaona zimene zinacitika ndi kucitapo kanthu mwamsanga . N’nali wonyada cifukwa ca luso langa loimba . Conco , n’nafunika kuphunzila kukhala wodzicepetsa . Ngati mukufuna kudziŵa zambili onani nkhani 12 m’buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa M’ceni - ceni lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova . N’cifukwa ciani webusaiti yathu ndi njila yothandiza kwambili polalikila ? Fotokozani zocitika za mu ulaliki zimene mwakhala nazo pogwilitsila nchito webusaiti yathu . Tingagwilitsilenso nchito pempho loyamba mpempheloli , kuonetsa anthu kuti Mulungu ali ndi dzina limene liyenela kuyeletsedwa . — Mat . 6 : 9 . Koma limenelo lidzakhala bodza . Mwacitsanzo , malamulo a Arabi anali kunena kuti anthu sayenela kuyandikila munthu wodwala khate mpaka kufika pa mtunda wa mamita aŵili . 25 : 2 , 3 , 25 ) Kwa kanthawi Davide ndi anthu ake anateteza katundu wa Nabala . Ngati ndinu wolapa moona mtima , ndipo munaulula macimo anu , musakayikile kuti Yehova anakukhululukilani . Kodi Mulungu ndiye acititsa ? A Zulu : N’zoona , timatelo . 11 : 1 ) Inde , cikhulupililo cimaphatikizapo kuyembekezela madalitso amene Mulungu analonjeza . Abale ambili akufunikabe kuti akhale akulu mumpingo wacikhiristu . Ndipo onse amene adzayenelela kugwila nchito imeneyi kutsogolo , afunika kupitilizabe kuphunzitsidwa . Mmodzi wa makasitoma ake anali Aksamai Sultanalieva , amene anali mkazi wa loya wa boma . Zinali zocititsa cidwi kuona cikondi na mgwilizano umene unali pakati pa abale na alongo ocokela m’maiko osiyana - siyana . Inoki anadziŵa kuti Yehova afuna kuti iye akhale wokhulupilika kwa mkazi wake . N’zoona kuti iye angamve kuŵaŵa cifukwa comenyedwa , koma kucita zimenezi kungapulumutse moyo wake . Kodi muona kuti Mulungu wakuthandizani m’njila ziti ? Lösch ) , 7 / 15 ( 1 Pet . 2 : 2 ) Coyamba , pemphani Yehova kuti akuthandizeni kukhala odzilanga nokha n’colinga cakuti muzipeza nthawi yophunzila Mau ake . 14 : 1 , 3 ; 22 : 17 ) Madzi ophiphilitsila amenewo akuimila zinthu zimene Yehova wapeleka kuti anthu amasuke ku uchimo ndi imfa pa maziko a nsembe ya dipo ya Kristu . ( Mat . 20 : 28 ; Yoh . 3 : 16 ; 1 Yoh . Pambuyo pake , anapatsako mwamuna wake pamene anali limodzi , ndipo nayenso anadya . ” Nyama zinalengedwa munthu asanalengedwe . Kucita zimenezo kunathandiza kuti cilakolako coipa cisazike mizu mumtima mwake . ( Deut . 15 : 4 - 6 ) Kodi mumakhulupilila na mtima wonse kuti Yehova adzakudalitsani mukapitiliza kum’tumikila mokhulupilika ? Mgwilizano wa mau a pa Salimo 144 : 12 - 15 na mau a m’mavesi a pambuyo umadalila mmene liu loyamba mu vesi 12 lamasulidwila . Mwana amene anali kutumikila ku Paraguay ndi mkazi wake anaganiza zosiya utumiki wao kuti akasamalile makolo . Onani Nsanja ya Olonda ya April 15 , 1991 , tsamba 21 mpaka 23 . Anthu amene anali kumumvetsela anali kudziŵa zimenezo . Kusacita zinthu mopitilila malile 3 : 7 ) Nkhani ya kucipinda siifuna kucitoumiliza kapena kulamula yayi . Ine na Arthur Matthews tinadziŵana mu 1946 . Umoyo unali wovuta cifukwa nthawi zambili pamalopo panali kukhala cimphepo ndi fumbi . ▪ Malo a Akazi m’Kakonzedwe ka Yehova Caka ca 537 B.C.E . cinali caka ca cikondwelelo kwa anthu a Yehova odzipeleka . ( Chiv . 4 : 11 ) Ndithudi , Yehova tiyenela kum’patsa ulemelelo na ulemu waukulu . Ndipo tingacite izi mwa kupeleka kwa iye zinthu zathu zabwino kwambili . Mukamaphunzila Baibulo , muzifufuza mfundo zimene zingakuthandizeni kudziŵa maganizo a Yehova ndi mmene amamvelela . Anali kuwauza kuti : “ Tiimbileni imodzi mwa nyimbo za ku Ziyoni . ” Muziseŵenzetsa kwambili Malemba M’madela ambili , anthu anali kudalila Baala kuti awateteze . Bwenzi laconco lili ngati Natani ndi Husai , amene anakhalabe okhulupilika ngakhale pa nthawi yovuta . Ndiponso bwenzi lotelo lingafanane ndi Yesu , amene anali wofunitsitsa kukhululuka . Komabe , atumiki ambili a pa Beteli anapanga masinthidwe amenewa . ( Luka 12 : 15 ) “ Dama ndi conyansa camtundu uliwonse kapena umbombo zisachulidwe n’komwe pakati panu , monga mmene anthu oyela amayenela kucitila . ” — Aefeso 5 : 3 . 6 : 16 ) Paulo analemba kuti anthu amene amapanga mtundu watsopano safunika kudulidwa , monga mmene zinalili ndi mbadwa za Abulahamu . Sindikaikila kuti Yehova anagwilitsila nchito M’bale Gardner ndi mlongoyo kuti andipatse malo okhala . Kukhululukila ena kumaonetsa kuti ndise acikondi ndi okoma mtima , ndipo kumalimbikitsa mgwilizano mu mpingo . Cinanso , kumatithandiza kuti tipitilize kuika maganizo athu pa mphoto ya moyo . Mwina poganiza kuti pathupi pakum’pangitsa kukhala wofunika kwambili kuposa Sara , Hagara anayamba kunyoza mbuye wake . Koma mukali kukaikila ngati mudzakhaladi osangalala mukakhala ndi ndalama zocepa ndiponso katundu wocepa . Adamu pofunsidwa na Mulungu , anakankhila mlandu kwa mkazi wake , amvekele : “ Mkazi amene munandipatsayu ndi amene wandipatsa cipatso ca mtengowo , ndipo ine ndadya . ” kudziŵa kuti Yehova amakukondani ? Mwacitsanzo , anakambilana momasuka ndi mkazi pacitsime pafupi na mzinda wa Sukari . ( Yoh . Timacita phunzilo limeneli ndi munthu aliyense payekha kapenanso m’tumagulu . Tili ndi udindo wouzako anzathu kuti nawonso angakhale pa ubwenzi ndi Mlengi wathu . ( Yobu 26 : 14 ) Koma ngati tiyesetsa kuphunzila zambili zokhudza iye , tidzakhala anzelu ndipo tidzapanga zosankha zabwino . Kapepala koitanila anthu ku mwambowo kanali ndi mau akuti : “ Anthu amene amakukondani adzakulandilani kuno . ” M’kupita kwa nthawi , David anaona kuti afunika kusintha , ndipo anasinthadi n’kukhala munthu wamtendele . Ngakhale kuti ena angaoneke ofooka , kodi io saonetsa kuti ndi okhulupilika ndi olimbikila ? Mneneli Amosi anafunsa kuti : “ Kodi anthu aŵili amayenda pamodzi asanapangane ndi kukumana mogwilizana ndi pangano lawolo ? ” Munthu wina kumeneko anamunyoza kangapo konse , koma iye sanaleke kulalikila . Zinali ngati kuti mzimu woyela ukum’kankha kuti apite kwina . ( Mac . Kupeza nthawi yosinkhasinkha pa zinthu zabwino zimene Yehova , Atate wathu wacikondi waticitila , kudzatithandiza kukhala ndi mtima woyamikila , ndipo tidzakhala anthu oyamikila nthawi zonse . — Ŵelengani Salimo 92 : 1 , 2 . Kamasulidwe katsopanoka kamagwilizana ndi malemba ena a m’Baibo amene amakamba kuti Mulungu adzadalitsa anthu okhulupilika . 8 , 9 . ( a ) N’ciani cingaonetse kuti timacitila tsankho anthu a mtundu wina ? Zimenezi zandithandiza kukhala womasuka kukambilana nao nkhani imeneyi . “ Doc ” McCartney anali kucitila upainiya . N’cifukwa ciani tikunena zimenezi ? Onani Nsanja ya Olonda ya April 15 , 2012 , tsamba 25 mpaka 26 . Pitilizani kucita khama kuti mupeze nzelu na malangizo ocokela kwa Mulungu , zimene ni cuma ca kuuzimu . Ngati muli ndi cikhulupililo , inunso mudzam’dziŵa bwino Yehova monga kuti mukumuona . Patangopita nthawi zinthu zomvetsa cisoni zinamucitikila Yosefe , munthu amene anali kukonda kwambili anamusiya . Nchito ya anthu a Yehova ikukulila - kulila , ndipo ikuloŵetsamo zambili . Umaonetsa kuti mwadzipeleka kwa Yehova , kutanthauza kuti mwamulonjeza kuti mudzamutumikila kwamuyaya . N’zinthu 4 ziti zimene zingatithandize kuwongolela kaimbidwe kathu ? Izi zinacititsa kuti Yehova am’kane . Mkhristu aliyense ali na ufulu wosankha mmene angadzitetezele , kapena mmene angatetezele banja lake ndi katundu wake . Alinso na ufulu wosankha nchito imene afuna . Ndinali kuganiza kuti kum’patsa zinthu zakuba monga ndolo ( masikiyo ) , mphete , ndi zibangili kunali kokwanila . Kodi n’ciani cinacitika Stephen atayamba kutsatila malangizo a m’Baibo ? Ena anali asanaonepo boti kapena mzungu . ( Aroma 16 : 1 , 3 , 6 , 12 ) Kwa nthawi yaitali , Nsanja ya Mlonda yakhala ikuchula Akhristu oona kuti ‘ abale na alongo . ’ Anamuuza kuti : ‘ Khala wolimba mtima ndipo ucite zinthu mwamphamvu . Cikondi ceniceni pa Yehova cozikidwa pa mfundo zake , cidzatithandiza kukhala odzicepetsa “ pansi pa dzanja lamphamvu la Mulungu . ” Komabe olo tiupeze , nthawi zambili sukhalitsa . Nanga malamulo amenewo anasiyana bwanji ndi amene Aisiraeli analandila ? ( Maliko 6 : 34 ) Anthu amene anatsatila ziphunzitso zake anasintha umoyo wao . CIFUKWA CAKE ENA AMAKAIKILA : Malinga ndi kafukufuku waposacedwapa , mlalang’amba wathu ukhoza kukhala ndi mapulaneti pafupifupi 100 biliyoni . Cinanso cimene cimatithandiza kukhala na mtendele weni - weni , ni mzimu woyela , umene ni mphatso yamtengo wapatali yocokela kwa Atate wathu wakumwamba . — Mac . 9 : 31 . Nanga nkhani yake itikhudza bwanji masiku ano ? Ndiyeno , Inoki anaona masomphenya ocititsa cidwi . Komabe , anthu amacita cidwi kwambili na paradaiso . Ndiyeno tibwelelenso ku mfundo yoyamba ija . Mofananamo , ngakhale kuti Mulungu simungamuone ndi maso anu , mukhoza kumuona pogwilitsila nchito “ maso a mtima wanu . ” Ndisanayambe kusinkhasinkha , ndimapemphela kwa Yehova kuti ndikhale ndi maganizo oyenela . Ngati tiyesetsa kulalikila molimba mtima ndi kugwilitsila nchito njila zatsopano polalikila , tidzayamba kudalila kwambili Yehova ndipo tidzakhala alaliki aluso . ​ — Ŵelengani 2 Akorinto 12 : ​ 9 , 10 . Koma bwanji za anthu ena amene anafa pa nthawi ina m’mbili ya anthu ? Ndinali kuwakonda kwambili ambuye anga makamaka aakazi , a Elisabeth . Mofananamo , ngati tiganizila kwambili za mavuto athu , tingayambe kukaikila kuti Yehova adzatithandiza . Ayi , tate wacikondi sangaganizileko zimenezo . Zinali kuthandizanso munthu wakupha mnzake mwangozi kupindula na cifundo ca Yehova . Nanga ena anawathandiza motani ? 10 : 30 ) Komanso , wamasalimo anati : “ Yehova amadziŵa za moyo wa anthu osalakwa . ” Mfundo za m’Baibulo zaniteteza komanso zanicititsa kukhala na umoyo wabwino kwambili . — Salimo 1 : 1 - 3 ( Mateyu 24 : 14 ) N’naphunzilanso kuti Akhristu oona sacita utumiki wawo kuti apezelepo ndalama . Kuti tim’thandize munthuyo kumvetsetsa nkhaniyi , tingam’funse kuti : “ Ngati Yesu asanafe anali wolingana ndi Mulungu ndipo pambuyo pake Mulungu anamukweza ndi kumuika pamalo apamwamba , kodi zimenezo sizikanacititsa Yesu kukhala wamkulu kuposa Mulungu ? Iwo anali kuphunzila Baibulo ndipo anali kucita zimene angathe kuti auzeko ena zimene anali kuphunzila . ( 1 Yoh . 2 : 15 - 17 ) Conco , tifunika kuyesetsa kuteteza cuma cathu cauzimu ndi kumaciona kuti ni cofunika kwambili . ( Ŵelengani Ekisodo 23 : 9 . ) 12 : 7 - 10 ) Kodi pamenepa iye anatanthauza ciani ? Zimene Yosefe anacita zingatilimbikitse kudzifunsa kuti , ‘ Kodi ndimasonyeza kuti ndimakhulupilila Mulungu mwa kudela nkhawa anthu ena ? ’ Ndipo ine na Tony taona kuti Yehova wakhala akutithandiza panthawi zovuta . Komabe pali umboni wosatsutsika woonetsa kuti tili pamapeto penipeni pa nthawi yapadela m’mbili ya anthu . Aliyense anali waubwenzi . ( b ) Kodi makolo angatengele bwanji citsanzo ca Yehova ? Ngati bodza limene ananama linacititsa kuti munthu wosalakwayo afe , wonamayo anali kuphedwa . Mwacionekele , mungamuyamikile dokotayo cifukwa cokuthandizani kuthetsa vuto lanu . Yesu anayelekezela uthenga wabwino wa Ufumu ndi mbeu imene yabyalidwa pa nthaka zosiyanasiyana . Anyamata amenewo anali okongola kwambili , anzelu , ndipo sizikanawavuta kutengela umoyo wa ku Babulo . Kodi mudziŵa kuti mungapindule mukamvetsetsa tanthauzo la masomphenya amenewa ? Lemba la Genesis 7 : 3 limakamba kuti analowetsa nyama m’cingalawa “ kuti zisungike padziko lonse lapansi . ” Ndimaonabe kuti utumiki ndi mwai wanga wamtengo wapatali . Tonse Timafunika Citonthozo 3 Cioneka kuti Demetiriyo amene , ndiye anapeleka kalatayi kwa Gayo . Ndipotu Yehova anatiikila lamulo lakuti , ‘ Ndakuikani monga kuwala kwa anthu a mitundu ina , kuti mukhale cipulumutso mpaka kumalekezelo a dziko lapansi . ’ ” ( Mac . Cifukwa cakuti zosankha zimene tingapange , zingakhudzenso zosankha zina . Panthawi imene Davide anali kuthawa , Husai anapita kwa iye . Kungafeŵetse mtima wa munthu wokwiya . Kodi anaphunzitsa bwanji otsatila ake kupewa tsankho na kukhala ogwilizana ? Makolo anga onse anafa ali okhulupilika kwa Yehova , ndipo niyembekezela mwacidwi kudzawalandila m’dziko labwino latsopano . Komabe , n’zolimbikitsa kudziŵa kuti Yehova adzapitilizabe kukonda “ anthu ake ” amene amatsatila njila zake zolungama . — 2 Tim . 2 : 19 ; ŵelengani 2 Mbiri 16 : 9a . Cifukwa n’nali kucilikiza mfundo yakuti anthu onse ni olingana . ( Aheb . 4 : 16b ) Nthawi iliyonse tikakumana ndi ciyeso kapena mavuto ena , tingapemphe Yehova kuti atithandize . Ngakhale kuti ndife ocimwa , iye amayankha mapemphelo athu . Iye anaona kuti abale kumeneko anali otangwanika kwambili na zinthu zaumwini . Patangopita milungu yocepa Yesu atabwelela kumwamba , ophunzila ake anazunzidwa ndi kuopsezedwa ndi otsutsa . ( 1 Mbiri 28 : 20 ) Zimene atate wake anakamba zinam’limbikitsa kwambili Solomo , ndipo anakwanitsa kugwila nchitoyo ngakhale kuti anali wamng’ono ndi wosakhwima . ( Luka 22 : 24 , 33 , 34 ) Komabe , Yesu anawayamikila atumwi ake okhulupilika cifukwa cosamusiya panthawi ya mayeselo . Iye anakambilatu kuti iwo adzacita nchito zambili kuposa iye . Kucita zimenezo ‘ kungationonge ’ mwakuuzimu . Ni mafunso ati amene angatithandize kudziŵa ngati timakonda zosangalatsa moyenela ? Simone na Anna Zosangalatsa n’zakuti ana athu onse atatu anayamba upainiya atatsiliza sukulu . Patapita caka cimodzi cabe , ninayenda ku Ghana kukatumikila monga mpainiya . ” Koma ubwino ni wakuti Yehova sacita nafe “ mogwilizana ndi macimo athu . ” Mwina simungakwanitse , ndipo n’kutheka kuti simunaionepo . ( Ŵelengani Macitidwe 16 : 14 , 15 ; Afilipi 4 : 15 - 18 . ) Tinapanga masinthidwe amenewa cifukwa cokonda Yehova , ndiponso cifukwa cakuti iye anatithandiza kucita zimenezo . Pamene Mose anakamba mau amenewa sanali kukamba za ciphunzitso cabodza ca utatu . Natani anayamba kukamba mwafanizo chimo limene Davide anacita . SOLOMO analangizidwa kuti ayang’anile nchito yofunika kwambili yomanga imene inali isanacitikepo n’kale lonse . Kukumbukila zinthu zabwino zimene tili nazo panthawiyo , kungatitonthoze ndi kutilimbikitsa . Iye anayembekezelabe zotsatilapo zake zabwino . N’zoona kuti cifukwa ca kupanda ungwilo kumene tinatengela kwa makolo athu , nthawi zina timakhala na zilakolako zoipa . Pamene Yesu anali kukamba na Marita , kodi anali ataukitsapo kale ndani ? Kukamba zoona , “ Tatenai bwanamkubwa wa kutsidya lina la Mtsinje , ” sanacite zambili . Conco , Venecia anayamba kuphunzila nawo . Marilyn anauza Jimmy kuti anapita kukagwila nchito pofuna kupezela iye zinthu zofunika . Ngakhale ngati zimene timacita pom’tumikila zingaoneke zocepa , Mulungu amayamikilabe na kutidalitsa , malinga ngati timazicita na mtima wonse , komanso cifukwa comukonda . — Maliko 12 : 41 - 44 . Ni lamulo liti limene Mulungu anapeleka kwa makolo athu oyamba ? Nanga colinga cake cinali ciani ? Mosataya nthawi , anabatizika . Ngakhale kuti muli ndi mphamvu zocepelapo tsopano , mukali ndi mwai waukulu wophunzitsa acinyamata . Mfumu Solomo anati : “ Mwana wanga , tamvela malangizo a bambo ako , ndipo usasiye malamulo a mayi ako , ” ( Miy . ( Akol . 3 : 15 ) Nthawi zina , cifukwa copanikizika na mavuto , tingaiwale kumuyamikila Mulungu pa madalitso ambili amene watipatsa . Kodi Yehova anayankha pemphelo limeneli ? Ici cinali cilengezo cofunika kucitapo kanthu mwamsanga . ( mogwilizana ndi Informant , * ya December 1937 , ya ku London ) Nkhaniyo inalinso ndi kamutu kakuti : “ Ciŵelengelo Sicikuwonjezeka pa Zaka 10 Zapitazi . ” Izi n’zimene Mulungu anacitila Rute . Ena mwa iwo anapita kale . Kodi muganiza kuti iwo akanakhalapo , sembe akutangwanika tsiku lililonse kuika mapikicha pa intaneti , kapena kuona zimene anthu ena amene si Mboni aikapo ? ( b ) Ndipo Asa anaunyalanyaza motani ? Nanga panali zotsatilapo zotani ? Pozunzidwa , timapilila . Ponyozedwa , timayankha mofatsa . ” — 1 Akor . Katswili wina wofufuza wochedwa Nate Silver , amagwilitsila nchito malipoti ocokela kwa anthu kuti am’thandize kulosela zilizonse monga mmene ndale zidzayendela m’dziko la U.S . , kapena amene adzalandila mphoto pa zamafilimu a ku Hollywood . Musaiŵale kuti mapemphelo anu ocokela pansi pamtima na ufulu wanu wokamba na Mulungu ‘ zidzabweletsa mphoto yaikulu kwambili . ’ ( 1 Yohane 5 : 19 ) Kodi Satana adzapitiliza kucititsa mavuto amenewa mpaka liti ? Ŵelengetselani mtengo . Tifunika kuunika mfundo yofunika pa lembalo , mwina mwa kuŵelenganso mau amene agwilizana kwambili na mfundoyo , kenako n’kufotokoza tanthauzo lake . Timakhalabe okhulupilika kwa Yehova : Timakonda Yehova ndi kumumvela nthawi zonse . Sukulu ya Giliyadi inatiphunzitsa zinthu zambili zotithandiza ‘ kukhala zinthu zonse kwa anthu osiyanasiyana . ’ ( 1 Akor . Yesu anali kukonda kwambili anthu . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Muzimvetsela mwachelu kwambili . ” — Luka 8 : 18 . Tili ndi zifukwa zotani zimene zimaticititsa kukhulupilila kuti tikukhala m’masiku otsiliza ? M’malo mwake , tifunika kupempha thandizo . Mukamayesetsa kukhala munthu wabwino , iye amaona ndipo amayamikila ngakhale kuti nthawi zina mungalakwitse . Muziganizila zimene Yehova amafuna osati zimene anthu ambili amakonda m’dzikoli ( Onani ndime 15 ) N’nayamba kuiona molakwika nkhani ya kugonana . 2 : 26 ) Nanga tingacitenji tikadziŵa kuti talola maganizo athu ndi zokhumba zathu kutengeka ndi kusiyana ndi zimene Yehova afuna kuti ticite ? NKHANI YA PACIKUTO | N’CIFUKWA CIANI ZINTHU ZOIPA ZIMACITIKILA ANTHU ABWINO ? Mayankho a mafunso amenewa ali m’nkhani ziŵili zimenezi . Ndipo mu 1995 , anthu obwela ku msonkhano anauzidwa kuti azinyamula zakudya zao . M’masiku amenewo , ambili a ise tinali kulabadila mwamsanga tikaphunzila mfundo zoyambilila za coonadi ca m’Baibo . Conco mungafunse kuti : ‘ Kodi izi zingacitike bwanji ? M’bale Hughes anatifotokozela mavuto amene abale anali kukumana nawo polalikila Akatolika m’dziko la Irish Republic . Ngati zimenezi zingapitilize , pangakhale mavuto aakulu . M’nkhani ino , tidzakambilana zitsanzo za anthu ena amene anali kudziona kuti ali kumbali ya Yehova , koma panthawi imodzi - modzi anali kucita zinthu zom’khumudwitsa . Nthawi zonse n’nali kupemphela kwa Yehova kuti apitilize kunithandiza . Nanga tingatengele bwanji citsanzo cake ? Muyenela kukhala na colinga mu umoyo wanu . Izi zidzacititsa kuti cikhale cosavuta kumvetsetsa malangizo ake ndi kuwatsatila . Cifukwa cakuti timakonda abale ndi alongo athu mocokela pansi pamtima . N’zomvetsa cisoni kuti masiku ano , ngakhale ana aang’ono ali pangozi yoonelela zamalisece ndi zinthu zina zoipa . Malangizo ena afotokozedwa m’kabokosi patsamba lino . Monga mmene Yesaya ndi Mika analoselela , tikukwela “ phili la Yehova ” mogwilizana . ( Machitidwe 5 : 29 ; Tito 3 : 1 ) Kodi tingacite bwanji zimenezi ? Cikondi cimene ananionetsa cinanilimbikitsa kukhala na zolinga zauzimu . Ena a iwo sanafufuze mosamala kuti adziŵe ngati Mulungu alikodi . Koma amasankha kusakhulupilila Mulungu cifukwa coganiza kuti adzakhala na ufulu wocita zilizonse zimene afuna . ( b ) Fotokozani citsanzo coonetsa mmene nchito yathu yofesa mbewu za Ufumu imakhudzila anthu amene amationa . Nanga bwanji kwa makolo okhulupilika amene ana awo anapanduka ? Koma ngakhale tsopano timadziŵa kuti pali mbali zina zing’onozing’ono zimene tifunika kusintha kuti titengele Mulungu ndi Kristu . Pa zocitika zonsezi , tiyenela kudzisankhila zocita . Magazini imeneyi ikupezeka m’zinenelo 254 ndipo makope pafupifupi 59,000,000 amasindikizidwa mwezi uliwonse . Pamene tiŵelenga nkhani zimenezi , timayamba kumvetsetsa coonadi ca m’Baibulo ndi kucikonda kwambili . N’ciani cingatithandize kusankha bwino zovala ? Atadutsa panthaka youma pakati pa mtsinje wa Yorodano , io anapitiliza ‘ kuyenda akumalankhulana . ’ Mtumwi Petulo , mwamuna wokwatila , anakamba za Sara kuti anali citsanzo cabwino pankhani yolemekeza mwamuna wake . Adria na George Cifukwa cakuti abale athu sanatengeko mbali m’ndale , nyumba zao zinatenthedwa Conco , kulibe angakambe motsimikiza kuti ngati mzimayi amaseŵenzetsa ma IUD okhala na kopa , kapena mahomoni , n’zosatheka mimba kukhala . Mu 1919 , kagulu kocepa ka Ophunzila Baibulo kanasankhidwa kukhala “ kapolo wokhulupilika ndi wanzelu . ” Pamene nkhondo ya ku Korea inayamba mu 1950 , ndinalamulidwanso kuyamba usilikali . N’cifukwa ciani anasankha kuphunzila za Davide ? Mlongo wina dzina lake Ruth anati : “ Ena anathaŵa nafe limodzi kupita ku dziko lina , koma pambuyo pake analoŵa m’cipani ndi kubwelela kwao cifukwa cakuti sanafune kukhala mumsasa wa othaŵa kwao . ” M’kupita kwa nthawi , M’bale Russell anayamba kufalitsa magazini yochedwa Zion’s Watch Tower . 16 : 23 - 25 ) Paulo na Sila anapeza mphamvu mwa kuganizila za ciyembekezo cawo . Kuwonjezela apo , anakhalabe acimwemwe podziŵa kuti anali kuvutika kaamba ka dzina la Khristu . Pambuyo pa zaka zingapo , mu 1972 ine ndi Maxine , tinapita ku Beteli ya ku Brooklyn . Tinangoona mlongo wina amene anasiliza maphunzilo a Sukulu ya Gileadi akubwela kwa ife . ( Mat . 28 : 19 ) Cikanakhala kuti zimatanthauza ophunzila amene timapanga , ndiye kuti atumiki okhulupilika amene sakhala na mwayi wopanga ophunzila cifukwa colalikila m’gawo louma , akanakhala ngati nthambi zosabala za m’fanizo la Yesu . N’ciani cinacititsa Timoteyo kukhala mkulu wa citsanzo cabwino ? Kodi iye amaona kuti anadziikila colinga cabwino na kupanga cosankha coyenela pamene anali mtsikana ? Odzozedwa amasambitsidwa ndi “ mau a Mulungu . ” Ndipo amafunika kutsatila ziphunzitso za Kristu ndi mtima wonse paumoyo wao . ( Aef . Mwacitsanzo , pophunzitsa munthu kuti Mulungu ndi wamkulu kuposa Yesu , tingagwilitsile nchito fanizo ili : Coyamba , tinganene kuti ubale umene ulipo pakati pa Mulungu ndi Yesu tingauyelekezele ndi ubale wa Atate ndi Mwana . N’ciani cinalimbikitsa Yesu kucita cozizwitsa colembedwa pa Mateyu 14 : 14 - 21 ? 119 : 99 . ( Sal . 45 : 3 ) Koma nthawi idzafika pamene mfumu idzasolola lupanga lake ndi dzanja lamanja ndi kuligwilitsila nchito . Cifukwa ciani ? Solomo anafotokoza kuti : “ Pa anthu 1,000 , ndapezapo mwamuna mmodzi yekha woongoka mtima , koma pa anthu onsewa sindinapezepo mkazi woongoka mtima . ( Aheb . 13 : 6 ) Kudalila kwambili Yehova kunam’thandiza Paulo kupilila mavuto pa umoyo wake . “ Lankhulani molimbikitsa kwa amtima wacisoni , thandizani ofooka , khalani oleza mtima kwa onse . ” Mlonda amavutika kwambili na tulo kukatsala pang’ono kuca . Amayesetsa kuti akhaleko na umoyo wabwino , koma nkhondo , masoka a zacilengedwe , na matenda , zimasokoneza mapulani awo nthawi na nthawi . ( Sal . 46 : 1 ) Ndithudi , tili ndi zifukwa zambili zokhalila oyamikila ndi mtima wonse monga mmene wamasalimo analembela kuti : “ Yamikani Yehova , cifukwa iye ndi wabwino . 43 : 10 ) Ndithudi , muzapeza cimwemwe cacikulu mukapitilizabe kukhala wacangu mu utumiki . Mboni za Yehova zimene zinali m’maiko onse olamulidwa na Soviet Union , sizinali kutengako mbali m’zocitika zandale . ( Yoh . ( Aheb . 6 : 15 ) Potsilizila pake , Mulungu Wamphamvuyonse anadalitsa kwambili munthu wokhulupilika ameneyu . Makolo athu anaticitila zambili ndipo ndine wosangalala kuti ndimawasamalila tsopano . ” Ndinalibe mnzanga wolalikila naye , koma ndinayamikila kwambili thandizo la mlongo wina dzina lake Gertrude Lobner , amene anali kutumikila monga wothandiza mtumiki wampingo . Kodi dzina la Mulungu lingatanthauzenji ? Kodi mkulu angathandize bwanji m’bale kukula kuuzimu ? Anapatsidwa dzina loyenelela lakuti Isiraeli , ( kutanthauza “ Wolimbana ndi Mulungu ” kapena kuti “ Mulungu Walimbana Nawe ” ) . Kodi Baibulo limatithandiza bwanji posankha zosangulutsa ? Ngakhale n’conco , tifunika kusankha njila yabwino yowapililila . “ Monga mmene mwakhalila omvela nthawi zonse , . . . pitilizani kukonza cipulumutso canu , mwamantha ndi kunjenjemela . ” — AFIL . Panthawi ina , kutumikila Yehova sikunali kum’sangalatsa . Makhalidwe amenewa ni ofunika kwambili kuti munthu akapulumuke . ( Mat . Pofotokoza mmene zinthu zinalili pamene anayamba utumiki wa umishonale , m’bale wina anati : “ Tinali acicepele osadziŵa zambili , ndipo tinali kuyewa ku nyumba . Cofunika ni kukhala cabe pa unansi na Mulungu . ” ( Onaninso bokosi yakuti “ Mau Otsitsimula ndi Otonthoza . ” ) A Zimba : Cabwino . 3 Colinga ca Yehova Cidzakwanilitsika Koma , kwa zaka zambili , n’nali kubwela ku nyumba nili osasangalala cifukwa ca mavuto a ku nchito . Palibe aliyense amene anafuna kutelo , ndipo mmodzi wa iwo anacita kutiuza kuti : “ Ise Machainizi sitigulitsa malo , koma timagula . ” Kodi tidzamvetsela na kucitapo kanthu pa uthenga wabwino umene ukulalikidwa padziko lonse lapansi ? Pambuyo pake , anali kulengeza mumpingo za kuikidwa kwao . Mwacitsanzo , Petulo mmodzi wa atumwi 12 , analimbikitsa Akristu anzake kuti akhale ‘ omvela coonadi ndi kukonda abale mopanda cinyengo . ’ Cifukwa ca cakudya cimeneci , timakhalanso ophunzitsidwa bwino ndiponso okonzekela kucita nchito yofunika kwambili padziko lapansi imene ndi yolalikila . Mulungu wokhulupilika , amene sacita cosalungama . Samueli atamva kuti Aisiraeli akufuna mfumu , anakhumudwa ndipo anaona kuti anthu ake amukana . ( 1 Sam . Kumeneko anakumana ndi Mboni za Yehova , ndipo anayamba kuphunzila Baibo . Kukamba zoona , sayansi yayankha mafunso akuti “ bwanji , ” monga akuti : Kodi maselo a ubongo amaseŵenza bwanji ? Baibo imakamba kuti : “ Yehova anayala maziko a dziko lapansi mwanzelu . Nkhani yaciŵili idzafotokoza mmene tingalimbitsile cikhulupililo cathu mwa kukhala otsimikiza na mtima wonse kuti Mulungu amadalitsa anthu amene amam’funa - funa na mtima wonse . ( Miyambo 20 : 19 ) Komanso munthu wina akatikhumudwitsa , cingakhale canzelu kudziletsa osakamba ciliconse . — Salimo 4 : 4 . ( b ) Kodi ndi lonjezo lotani lokhudza ufumu limene Mulungu analonjeza Davide ? ( Luka 15 : 11 - 24 ) Atakumana ndi mavuto , Mwana wolowelelayo anazindikila kuti analakwitsa kucoka pakhomo pa makolo ake . Yesu , monga “ Kalonga Wamtendele , ” adzakhazikitsa mtendele ndi citetezo padziko lonse lapansi . Mwacitsanzo , tikafika tinali kufunsa kuti , “ Kodi pali aliyense amene agulitsako ng’ombe ? ” ( Ŵelengani Yakobo 5 : 13 - 15 . ) “ N’zosavuta kukhala oona mtima ngati zonse ziyenda bwino . Ndinazindikila kuti ndapezadi ubale wa padziko lonse . Kukhala ndi bwenzi lokonda Mulungu kungatithandize kupilila zoipa . Patapita zaka 5 , iye anakwatiwa ndi mkulu . Kucokela kale , anthu akhala akuyesayesa kugonjetsa imfa , koma zimenezi zalepheleka . Ndithudi , kodi si zotonthoza ‘ kutulila Yehova nkhawa zathu ’ podziŵa kuti ‘ adzaticilikiza ’ ? Aliyense amene amakonda kukhala kudela la mapili angamvetsetse kuti zinali zovuta kwa abale kucoka ku nthambi ya ku Switzerland , imene inali m’dela la mapili okongola . Ngati mumamvela conco , yesetsani kucita zinthu zoonetsa kuti mumaona kukhulupilika kwanu kwa Yehova kukhala kofunika kwambili kuposa cikondi ca pacibululu . N’nali kungoganizila za tsogolo langa . Pewani zinthu zosokoneza n’colinga cakuti muike maganizo anu pa zimene muŵelenga . Timaona kuti msonkhanowo unali wofunika kwa tonsefe m’Malawi cifukwa unatikonzekeletsa zimene zinali kudzacitika mtsogolo . Koma cikhumbo cofuna kuthandiza anthu amene amafuna kudziŵa Yehova cinakula . Pokamba na munthu amene si wacipembedzo cacikhristu , tinganene kuti , “ Onani zimene Mau Opatulika amakamba . ” Jowana anali kugwilizanabe ndi Yesu komanso ophunzila ake mosasamala kanthu kuti anali kucitilidwa zacipongwe ndi acibale ake , anzake ndiponso atsogoleli acipembedzo . 3 : 16 ; Mac . 16 : 25 . M’nkhanizi , tidzakambilana kufunika kokhala ndi dzina lakuti Mboni za Yehova . Tingatsanzile bwanji cikondi ca Mulungu pocita zinthu ndi anthu otelo ? Mwa ici , Aroma anamupha Yudasi . Afunika kupitiliza kulimbitsa cikhulupililo cawo mwa Mulungu ndi kumudalila kuti adzawasamalila . Takamba izi cifukwa m’caka ca utumiki ca 2015 , ofalitsa 8,220,105 analalikila uthenga wabwino mwakhama . Anthu ena anali kuwaona kuti ndi osaphunzila . Ngati museŵenzetsa malangizo a m’Baibo mudzapeza mabwenzi abwino amene angakuthandizeni ( Rute 1 : 16 ) Timakhudzidwa mtima tikaganizila mmene Rute anali kukondela Naomi . Ŵelengani . ) Kodi tiphunzilapo ciani pa “ cidindo ” ca m’fanizo la Paulo ? Musacite ciliconse ndi mtima wokonda mikangano kapena wodzikuza , koma modzicepetsa , ndi kuona ena kukhala okuposani . Musamaganizile zofuna zanu zokha , koma muziganizilanso zofuna za ena . ” — Afil . Pamapeto pake , ndinawauza kuti : “ Cabwino , tingayambe kuphunzila ngati mundilola kuseŵenzetsa Baibulo langa . ” Koma pamene Mfumukazi Yezebeli anafuna kumupha , anacita mantha . 3 : 8 ) Kukhala ndi cimwemwe cacikulu tikapeza coonadi kudzatithandiza kudzimana zinthu zina ndi kukhala wotsimikiza mtima kuika coonadi patsogolo pa umoyo wathu . • Ngati kuli Mulungu wamphamvuyonse , n’cifukwa ciani samateteza anthu abwino ku mavuto ? Tikhale Ogwilizana Pamene Mapeto a Dzikoli Ayandikila Masiku ano , anthu amaonetsa mzimu wonyada m’njila zambili . ( Yobu 42 : 1 - 6 ) Asanapatsidwe uphungu na Mulungu , Yobu anali atalandilapo kale uphungu wina wopelekedwa na Elihu . Ndipo ana onse aamuna a Levi anayamba kusonkhana kwa Mose . ” — Eks . Kulamanja : Thierry Iwo anapita ku Madagascar mu 2006 . ( Gen . 4 : 3 , 4 ) Nayenso Nowa anaonetsa kuti anali kukondadi anthu mwa kuwalalikila uthenga wa Mulungu kwa zaka zambili , ngakhale kuti sanali kulabadila . N’zoonekelatu kwa onse opezeka ku mwambowo kuti aŵiliwo akukondana kwambili . Patapita nthawi yocepa , mlongosi wanga wamkulu , Lucy , nayenso anamwalila ali na zaka 17 . Iye analandilidwa ndi Betuele , atate ake Rabeka . Iye ayenela kuti anafika pafupi kwambili na wonyamula cishango cake . Ngakhale kuti moyo wake unali pangozi , iye analankhula molimba mtima conco kuti ateteze ophunzila ake . 17 : 14 ; 20 : 10 . Kuyambila mu 1935 , otsalila a odzozedwa athandiza anthu mamiliyoni ambili “ kukhala olungama . ” Munthu amene amatha kuona mmene mfundo imodzi imagwilizanila ndi inzake timati amamvetsa zinthu . * Kodi inunso munakhudzidwapo na Malemba amene anagwilitsidwa nchito pa misonkhano yathu , kaya yampingo , yadela , kapena yacigawo ? — Neh . Tsiku lina , mlongoyu anakamba mokhadzula kwa mlongo amene anali kuseŵenza naye . Kodi ana amakhudzidwa bwanji ngati kholo likhala kutali ? Iye anali na mtima wofunitsitsa kucita zinthu mogwilizana ndi cifunilo ca Yehova , moti anabatizika mosazengeleza . Ena amaona kuti zimathandiza kuima pambuyo poŵelenga mavesi ena , n’kudzifunsa mafunso monga awa : ‘ Kodi zimenezi ziniphunzitsa ciani ponena za Yehova ? Pamene musankha zosangulutsa , mufunika kusamala kuti mupeleke citsanzo cabwino kwa ana anu . Pa utumiki wake wonse ali pano padziko lapansi , Yesu anali kunyozedwa ndi anthu acipembedzo . N’cifukwa ciani timayamikila ngati ena alemekeza nthawi yathu ? Popeza kuti Gayo anali kale woceleza , n’cifukwa ciani Yohane anamuuza kuti apitilizebe kuceleza alendo ? N’ciani cinathandiza amuna na akazi akale kuyembekezela Yehova moleza mtima ? Koma n’naganiza kuti , ‘ Ngati Yehova aona kuti ningakwanitse , n’dzayesako . ’ 9 “ Pitani Mukaphunzitse Anthu a Mitundu Yonse Kuti Akhale Ophunzila ” Caciŵili , muziganizila mmene Yesu anaonetsela cikondi ngakhale pamene anali kunyozedwa . Woyang’anila woyendela ameneyo anakamba kuti pambuyo pake amafunsa munthuyo kuti : “ Kodi munawaganizilapo mafunso awa ? ” Tiyenelanso kuganizila mmene tingalimbikitsile ofalitsa anzathu . Onaninso nkhani yakuti “ Kodi N’kuphonya Cabe pa Kamvedwe ? ” Kodi tingakambe kuti mfundo zina za coonadi ndi “ zakale ” m’lingalilo lotani ? Mdyelekezi amatiyesa ? Mwacitsanzo , kodi mumayesetsa kukhala oona mtima m’zinthu zonse ? ( Onani palagilafu 8 - 10 ) Pambuyo pa zaka zambili , anyamata anai aciheberi anasonyeza kuti anali kudziŵa cimene cinali cofunika kwambili . N’cifukwa ciani tiyenela kutengela cikondi ca Yehova ? Koma pamene ndinakhudzidwa kwambili ndi imfa m’pamene mtima wanga unasangalaladi ndi zimene zidzacitika cifukwa ca dipo lamtengo wapatali limenelo . ” 6 : 1 - 5 . “ Mulole Kuti Kupilila Kumalize Kugwila Nchito Yake , ” Apr . Akristu enanso oyambilila amene anali omvela ndi okhulupilika anali kupewa kugwilizana ndi anthu osamvela Mulungu ndipo anapulumuka ciwonongeko ca Yelusalemu mu 70 C.E . — Luka 21 : 20 - 22 . N’zolimbikitsa kumvela nkhani za anthu amene anacitila ena zabwino . Pambuyo pake iye anati : “ Lekani ndikuuzeni cinthu cimodzi . Iye anakana kuthandiza Davide , ndipo anayankha anyamatawo mwamwano ndi monyoza . Popeza kuti anali kukhulupilila Yehova , “ Woweluza wa dziko lonse lapansi , ” iye anamuuza nkhawa imene anali nayo . Tingapemphele kwa iye ndipo adzatimva kulikonse kumene tili cifukwa “ iye sali kutali ndi aliyense wa ife . ” — Macitidwe 17 : 24 - 27 . Kodi tonse tingacite ciani kuti tizilimbikitsana wina na mnzake ? Mfundo imeneyi ingakhudze cikumbumtima ca Mkristu ngati iye angasankhe kulandila tuzigawo tung’onotung’ono twa magazi , tumene tumacokela ku zigawo zinai zikuluzikulu za magazi . Kodi cofunika n’ciani kuti dzina la Mulungu liyeletsedwe kothelatu ndi kucotsedwa citonzo ciliconse ? Akatswili ena amakhulupilila kuti Abulahamu ananyamula mtsuko kapena poto wonyamula ndi cheni . M’potomo munali malasha oyaka moto kapena makala amene anapalidwa pamoto wocezela usiku . ( Yes . Iye anati : “ Mkazi wanga anamwalila zaka 7 zapitazo , koma ndisaname , imfa ndi yopweteka . Petulo anali ndi cikhulupililo colimba . ( 1 Maf . 18 : 21 ) Palinso anthu ena amene anasiilatu kugwilizana ndi mpingo wacikristu . Zimenezi n’zofunika cifukwa ciani ? Kuyambila nili mwana , n’nali kuopa imfa . Koma sanali kuwalangiza mwamphamvu . Ngati n’conco , pemphani wa Mboni za Yehova kuti muziphunzila naye Baibulo kwaulele . . Akanipeza , amayi anali kuvutika kwambili na cisoni ndipo anali kunitenga n’kuthamangila nane ku cipatala . 31 : 19 ; 32 : 4 . Ise ana tinali kulemekeza Baibo , koma pamene tinali kukula tinayamba kucenjenekewa na zosangulutsa . Kuti tione kufunika kwa mfundo imeneyi , tiyeni tikambepo za nkhani ina yodetsa nkhawa imene imakhudza makolo ambili . Nthawi ina ndinapempha kuti ndizigwila nchito maola 36 pa mlungu , kutanthauza kugwila nchito maola 6 kwa masiku 6 . Popeza “ Nowa anayenda ndi Mulungu woona , ” Yehova anam’patsa malangizo akuti apange cingalawa cacikulu . Komanso mumadziŵa kuti Mau a Mulungu amatilimbikitsa “ kuphunzitsa ena . ” Zimenezi zingafanane ndi kusunga makiyi a galimoto . Amadzifunsa kuti : ‘ Kodi nivutikila ciani kufuna kukhala na umoyo wabwino ? ’ Steffen ( 2 ) Kodi Cikumbutso cimagwilizanitsa bwanji anthu a Mulungu ? 4 : 2 , 3 ) Kuti tikhululukile ena mocokela pansi pa mtima , tiyenela kupewa ‘ kusunga zifukwa . ’ ( 1 Akor . Nthawi zina anali kuyesa kusokoneza mapulogilamu athu mwa kuliza mabelo a chechi yawo akationa tikucita misonkhano kufupi nawo . ( Chiv . 22 : 5 ) Anthu amenewa ndi amene amadya zizindikilo pa mwambo wa Mgonelo wa Ambuye . ( Mateyu 10 : 34 - 37 ) Anandifotokozela kuti ndikakhala wokhulupilika kwa Yehova , acibale anga angathe kuphunzila za Iye . M’busa wabwino amafufuza mosamalitsa nkhosa iliyonse kuti atsimikizile ngati ili bwino . Mau ngati amenewa , okambidwa ndi anthu amene si Mboni amaonetsa kuti gulu lathu la abale padziko lonse n’lapadeladi . 105 : 13 , 14 ) Yehova anali wokhulupilika kwa bwenzi lake Abulahamu , ndipo anam’lonjeza kuti : “ Mwa iwe mudzatuluka . . . mafumu . ” — Gen . Ufumu wa Mulungu unalidi wofunika kwambili kwa Yesu . ​ — Ŵelengani Mateyu 12 :⁠ 34 . Phunzilo lija linapitiliza ndithu , ndipo ndinayamba kuona kuti ndifunika kusintha kwambili umunthu wanga . Panthawi ina Mose analephela kulemekeza Yehova . Zoonadi , kukonda utumiki kumatithandiza kuti tisagonje kwa anthu amene amatizunza . Claire anati : “ Tili ndi cimwemwe cacikulu cifukwa cotumikila Yehova tsiku lililonse . Nthawi ina , ine ndi atate anga opeza tinapitila pafupi ndi Nyumba ya Ufumu . M’Baibo , Yehova amam’kamba kuti ni Mulungu “ amene sanganame . ” Timayang’anitsitsa Yesu mwa kuŵelenga zinthu zimene anacita ndi kuphunzitsa , ndiponso kum’tsatila mosamala kwambili Mukacita zimenezo , mudzakwanitsa kupeleka mphatso imene idzamuthandiza pa cosoŵa cimene ena sanaganizilepo . Paulo anawayamikila , ndipo nayenso Yehova anawayamikila . ( b ) Kodi kukhala ndi nthawi za mtendele m’maiko ena kwathandiza bwanji pa nchito yolalikila ? Tili m’chechi pa Sondo , mokwiya wansembe anati : “ Mwaliona buku ili ! ” Citsanzo ca Gagik cionetsa kuti mfundo imeneyi ni yoona . Kodi mabanja ena amacita ciani kuti acititse kulambila kwa Pabanja kukhala kosangalatsa ? Conco , cinali covuta kwa anthu kukhala okhulupilika kwa Mulungu popeza mfumu imene inasankhidwa kuti ikhale “ pampando wacifumu wa Yehova , ” inali kucita zoipa . — 1 Mbiri 29 : 23 . ( Aef . 5 : 23 ) Yesu amacita umutu wake mwacikondi ndi moleza mtima pa mpingo . Mukalimbikila , mungazikwanilitse Zimene Baibulo limanena zokhudza mapeto a dziko ndi nkhani yabwino Ena amakamba kuti khalidwe lonyada n’loipa kwambili cakuti olo anthu onyadawo amaipidwanso na anthu anzawo onyada . 15 : 32 ) Sitimaika maganizo athu pa zosangulutsa , m’malo mwake timayamikila ciyembekezo ca ciukililo . Ngati muli ndi mafunso ofanana ndi amenewa , kodi mayankho ake mungawapeze kuti ? Kodi mafanizo angathandize bwanji ana anu kukhulupilila Baibulo ? Mungaonanenso na Mboni za Yehova kufupi na kwanu kapena kupita ku Nyumba ya Ufumu m’dela lanu . Ndi zinthu ziti zimene Mulungu afuna kuti tizicita monga anthu ake ? Ndipo salandila ciphuphu kuti akhotetse mlandu wa munthu wosalakwa . ” — Sal . Mulungu anam’patsa nzelu zambili komanso udindo womanga kacisi waulemelelo ku Yerusalemu . Yehova atatsala pafupi kuwononga mizinda yoipa ya Sodomu na Gomora , angelo anathandiza munthu wolungama Loti na banja lake kuthaŵa . — Genesis 19 : 1 , 15 - 26 . Ndinafunika kusintha maganizo anga kuti ndizicita zinthu mwamtendele komanso kuona kuti ndiyo njila yabwino kwambili yokhalila ndi moyo . Patapita nthawi , iye analemba kuti : “ Pa zinthu zonse , ndimapeza mphamvu kucokela kwa iye amene amandipatsa mphamvu . ” Mosasamala kanthu kuti alengezi a Ufumu amene anali ku France anabwelela kwao kapena anakhalilatu kumeneko , iwo akutsatila mwakhama citsanzo ca Olengeza Ufumu akale a ku Poland . — Za m’Nkhokwe Yathu ku France . Muzikhala kuno ku phili kuti muziyang’anila nkhosazi . ” Acinyamata — Kodi Ndinu Okonzeka Kubatizidwa ? Ngati tikuvutika kuthetsa cilakolako coipa , tiyenela kupempha thandizo kwa Akristu anzathu . Kutengako mbali pa nchito yolalikila kumatiteteza ku mlandu wa magazi . — Ezek . M’kupita kwa zaka , ambili a Akristu odzozedwa amenewa amaliza moyo wao wa padziko lapansi mokhulupilika . ( Num . 14 : 26 - 30 , 34 ) Conco , zimene Yehova anacita poweluza Mose kuti sadzaloŵa m’Dziko Lolonjezedwa cinali cilungamo , cifukwa nayenso Mose anaonetsa mzimu wopanduka . Ndithudi , tapindula kwambili kuphunzila mfundo zina za m’buku la Levitiko . ( Salimo 90 : 1 , 2 ) Ngakhalenso mneneli Yesaya anati : “ Kodi iwe sukudziŵa kapena kodi sunamve ? Samueli anafuna kugwilitsila nchito nthawi ya cakudya ndi maceza kuti athandize Sauli kukhala womasuka . 9 : 11 , 12 ; Yak . 4 : 13 , 14 ) Motelo cifukwa cokonda nkhosa za Yehova , akulu amene amaganizila zamtsogolo amaphunzitsako abale ena acinyamata zinthu zimene aphunzila pa nthawi imene akhala akutumikila Mulungu mokhulupilika . — Ŵelengani Salimo 71 : 17 , 18 . Iwo anaonetsa cikhulupililo mwa Yehova pamene anapita kukazonda Dziko Lolonjezedwa . ( b ) Kodi m’nkhani ino tidzakambilana ciani ? Koma kudzicepetsa sikutanthauza kuti sitingakalamile udindo kapena utumiki woonjezela iyai . N’nali kuona kuti io analibe Baibulo yoyambilila ndipo Baibulo imene anali nayo inasinthidwa . ” Baibo siifotokoza kuti cimene cinacititsa zimenezi ndi kusiyana zibadwa . Peter anayamba kusintha . 4 , 5 . ( a ) Ndi njila zothandiza ziti zimene zingathandize ana kumasuka ndi makolo ao ? Ndimawakonda kwambili akulu anga , a John ndi a Ron ndipo ndinawalalikila mowakakamiza . Ena amaganiza kuti akafa , adzapitiliza kukhala na moyo , mwina m’cinthu cina kapena kumalo ena . Ndife okhulupilika kwa Yehova ndi kwa anthu ake . Ena akatilakwila , sitileka kusonkhana ndiponso siticoka mumpingo . M’malomwake , iye analenga mkazi wangwilo , Hava , kuti akhale mthandizi wa Adamu . Lomba , tiyeni tikambilane mmene atumiki ena a Mulungu anatonthozedwela na Yehova , ndi mmene anapindulila na citonthozo cake . Pakati pawo panalinso munthu mmodzi “ atavala zovala zansalu ” ndipo anali ndi “ kacikwama ka mlembi , konyamulilamo inki ndi zolembela . ” 5 : 22 , 23 ) Monga mmene oilo imathandizila mashini kuseŵenza bwino , makhalidwe aumulungu amenewa amathandiza pokhazikitsa mtendele . Kuteteza Uthenga Wabwino Pamaso pa a Boma , Sept . Panthawi ina , Mboni pafupi - fupi 90 zinakagona ku ofesi ya nthambi . 6 : 1 , 4 ) Kodi izi zitanthauza kuti makolo ayenela kuikila ana awo m’ndandanda wa malamulo ? M’bale Morris anafotokoza kuti bukuli linakonzedwela “ anthu a ku Japan . ” 3 : 1 - 10 , 12 , 13 ; 1 Pet . Cikhulupililo cidzatithandiza kudziŵa kuti “ dziko likupita limodzi ndi cilakolako cake . ” ( 1 Yoh . Tsopano ganizilani umoyo wanu malinga na mau a Paulo akuti : “ Musalole kuti ucimo uzilamulilabe monga mfumu m’matupi anu okhoza kufawo kuti muzitsatila zilakolako zawo . ” Nanga zikanatheka bwanji kuti Ayuda ocepa akwanitse kugwila nchito yaikuluyo ? Ophunzila Baibo anaiona mfundo yake , yakuti sangakhale pa mgwilizano na ŵanthu okangamila ku cipembedzo conama . — Ŵelengani 2 Akorinto 6 : 14 . 1 , 2 . ( a ) Ni nkhani yaikulu iti imene ikhudza anthu onse ? Kodi Mau a Mulungu angatipatse bwanji mtendele wa maganizo ? Tiyeni tikambilane kusiyana pakati pa cikondi cogwilizana ndi mfundo za m’Baibo na cikondi cimene lemba la 2 Timoteyo 3 : 2 - 4 limakamba . Inga ndi Mikhail ‘ Ndodo yake yacifumu ndiyo ndodo yacilungamo . ’ Conco , ulamulilo wake udzakhala wosakondela ndiponso wacilungamo . Okhulupilila zakuthambo amaika anthu m’magulu 12 poseŵenzetsa zizindikilo za zinthu zakuthambo . Takamba zimenezi cifukwa ku United States kuli atsogoleli a Machalichi Acikristu okwana 600,000 , koma kuli Mboni za Yehova 1,200,000 zimene zimalalikila uthenga wabwino . ( Luka 22 : 32 ; Aheb . Nchito iliyonse imene akulu akupatsani muyenela kuigwila ndi mtima wonse . “ Tiyeni tidziyeletse ndipo ticotse cinthu ciliconse coipitsa thupi kapena mzimu . ” Ndiyeno analandila foni kucokela kwa mgwilizanitsi wa bungwe la akulu wa kumpingo wa makolo ao . Pamene ndinakhala kuseli kwa Nyumba ya Ufumu poyembekezela kuti ena abwele , ndinayamba kukumbukila zimene ndinaona ku Vietnam , monga magazi a anthu ndi cifungo ca mitembo ya anthu imene inali kutenthedwa ndi moto . Zimenezo zinandicititsa mantha . Ndiyeno , Mulungu anauza Aroni kuti sayenela kumva cisoni mwanjila iliyonse . Koma panthawiyo analimbikitsidwa kuwonjezela cangu cawo . 7 : 10 , 11 ) Kupatukana na mnzathu wa m’cikwati tisakutenge monga nkhani yopepuka . Tikukhulupilila kuti malangizo amene takambilana m’nkhani ino ndi m’nkhani yapita , athandize akulu kupeza nthawi yophunzitsa ena . Iye anati : “ Misonkhano imalimbitsa kwambili cikhulupililo canga . Makolo ake mwamsanga anayamba kum’thandiza kupanga mabwenzi abwino mumpingo . Tsiku lina pamene ine ndi m’bale wina wacikulile tinali kupita kukalalikila m’gawo na njinga , tinaona m’busa wacipembedzo . Mwacitsanzo , ndinathandiza munthu amene ndinali kudana naye ndili kusukulu ya sekondale , kuphunzila Baibulo . 32 : 28 , 29 . Khadi la ulaliki linathandiza ambili kuyamba kulalikila Abwana ake nawonso anali atayamba kuphunzila Baibo na Mboni za Yehova . Atanena mau amenewa , Paulo anagwila mau a pa Numeri caputala 16 , onena za kupanduka kwa Korah . KODI mudziŵako m’bale kapena mlongo amene anayenda ku dziko lina kumene kufunikila ofalitsa Ufumu ambili ? Aja amene amadela nkhawa nthawi zonse , sapeza cimwemwe cimene cimabwela cifukwa cotumikila Yehova . ” M’nthawi ya atumwi , kodi abale ndi alongo anatumikila Yehova m’njila ziti ? Muzigwilako nchito yothandiza anthu okhudzidwa na masoka . Cinthu cimodzi cimene cingakuthandizeni kukonda kwambili Yehova , ndi kuganizila mozama za dipo , limene ndi mphatso ya mtengo wapatali imene Mulungu anapatsa anthu . Pa ulendowo , M’bale Engleitner anafotokoza cikhulupililo cake mwaulemu kwa Gleissner , ndipo iye anamvetsela mwacidwi . Khalani onyadila kuti mwawaphunzitsa nchito acinyamata , ndipo aloleni lomba kuti atenge maudindowo . Ndipo mungasinkhesinkhe zimene Yesu anakamba ndi kucita . ( Aroma 10 : 17 ; Aheberi 12 : 2 ; 1 Petulo 2 : 21 ) Tilinso ndi cofalitsa cimene cimafotokoza zocitika pa umoyo wa Yesu motsatila nthawi imene zinacitika . Kuti apitilize kukhala ndi moyo , anafunikila kupuma , kumwa , kugona , ndi kudya . Nkhani ino ndi yotsatila , zalembedwela acinyamata amene afuna kubatizidwa Kakambidwe kawo , kavalidwe kawo , ndi zakudya zawo , zingakhale zosiyana kwambili ndi zanu . Njila yaciŵili imene tingalimbitsile mgwilizano ni kuganizila tanthauzo la zizindikilo za pa Cikumbutso . Ici n’cimodzi mwa zifukwa zimene ansembe aakulu na Afarisi anapangila ciwembu copha Yesu . Malinga ndi mapangano oona amenewa , sitikaikila kuti Ufumu umenewu udzapambana . Mwacitsanzo , nthawi ina pamene Yesu anapita kukawacezela , Marita anakhumudwa ndi mlongo wake Mariya . Iye anauza Yesu kuti am’langize . Carin anakambanso kuti : “ Kunena zoona , paciyambi ndinaona kuti panalibe vuto ndi kutumiza mwana wanga kwa makolo anga kuti akakhale naye zaka zocepa . Komabe , iye anapeza citonthozo mwa kuuza Yehova vuto lake m’pemphelo . M’mau ake otsiliza asanafe , iye anagwila mau a m’maulosi okhudza Mesiya . ( Mat . ( Aheberi 10 : 24 , 25 ) Tingasonyeze kuti timakonda abale athu mwa kupezeka pamisonkhano kuti tilimbikitsane . Coyamba , tifunika kutengela cikhulupililo ca akulu na citsanzo cawo cabwino . Tsopano Davide anadzionela yekha munthuyo . Ndaona mmene Yehova amandithandizila . N’cifukwa ciani Yehova analonjeza olambila ake mphoto ? Palibe afunika kukakamiza munthu kuti abatizike , kaya ni kholo , wophunzitsa Baibo , kapena wina aliyense mu mpingo . Mlongo ameneyu anathandizidwa ndi okhulupilila anzake . Kodi Ndi Zinthu Ziti Zomwe Tiyenera Kudziwa pa Nkhani ya Khirisimasi ? ” 3 : 19 ) Ndipo Yehova anamuuza kuti : ‘ Tsogolela anthuwa kumalo amene ndakuuza . Pokhulupilila za ciukililo sikuti Mkhiristu samvela cisoni cifukwa ca kutaikidwa munthu mu imfa . Kodi munthu wopha mnzake mwangozi anali kufunika kucita ciani kuti acitilidwe cifundo ? ( Aroma 11 : 33 ) Iye analola anthu kuyamba kudzilamulila okha kwa kanthawi , n’colinga cakuti aonetse kuti ndani ali woyenela kulamulila anthu . Kodi Davide analeka kucilikiza nchitoyo , cifukwa cokwinyilila kuti citamando comanga kacisi sicidzabwela kwa iye ? Iyai . Iye anali kuganizila mmene zokamba ndi zocita zake zingakhudzile ena . Abalewo anakondwela ngako kupezeka pa msonkhano wadela . Anaona kuti anacita bwino kwambili kucita zonse zimene akanatha kuti akapezekepo . Munthuyo pokhala Myuda , mwacionekele anali kudziŵa za Paladaiso wa pa dziko lapansi wochedwa munda wa Edeni , wochulidwa m’Baibulo . A Zulu : Cabwino , palibe vuto . Patapita masiku ocepa , azimai aŵili anabwela kunyumba kwathu . Kodi ndi zimene mumacita ? Iwo anali kukhulupilila Yehova na kum’dalila . ( Luka 10 : 1 ) Iwo anali kulimbikitsana pogwilila nchito limodzi . Mulimonsemo , Sara anali wofunitsitsa kupanga cosankha covuta cimeneci . 23 : 31 - 34 ) Ndiyeno m’bale wake , Yehoyakimu analamulila kwa zaka 11 . Tiyenela kukhala ‘ ocenjela ’ ndiponso anzelu mwa kupewa kukhulupilila zilizonse zimene munthu angatiuze , makamaka ngati munthuyo sanaphunzile zacipatala . Kucita zimenezi kudzathandiza kuti muone zinthu moyenela . Ngati n’conco , ndiye kuti mwacionekele mukufuna kukhomeleza khalidwe limeneli mwa ana anu . Kodi akulu ndiponso abale ena amene amaphunzitsidwa ndi akulu angaphunzile ciani kwa Samueli , Eliya , ndi Elisa ? Dzikoli limalimbikitsa kwambili “ cilakolako ca thupi , cilakolako ca maso ndi kudzionetsela ndi zimene munthu ali nazo pa moyo wake . ” Koma mkulu wina anandithandiza mmene ndingakonzekelele pemphelo ndi mmene ndingakhalile wodekha . Iye anakwanitsa kuphunzitsa bwino ana ake na kuwapatsa citsanzo cabwino , olo kuti kucita zimenezo kunali kovuta ngako m’masiku oipa amenewo Cigumula cisanacitike . — Gen . Ngakhale kuti zambili zimene amakamba zimacitika , zina sizicitika , ndipo zina zalephela mocititsa manyazi . Yesu sanangowapatsa mkate wocepa , koma anawapatsa cakudya cokwanila kuti onse akhute ndi kupeza mphamvu zoyendela mtunda wautali pobwelela kwao . Kodi mudzavomela ciitano ca Yehova cakuti muyende naye na kuti mukapeze madalitso osatha amene wasungila anthu amene avomela ciitano ? Titangoyamba utumiki umenewu , anatiitana kuti tikaloŵe Sukulu ya Utumiki wa Ufumu ku South Lansing , mumzinda wa New York . Panthawiyo , sukuluyi inali ya mwezi umodzi . Ndipo kuyambila mu 1948 kufika mu 1950 ciŵelengeloco cinali kuonjezeka kufika pa 20 ndi 23 , mpaka pa 40 peresenti . Gulu lathu likukulilakulila cifukwa cakuti timakhulupilila Mulungu , ndi kuvomeleza kuti Baibulo ndi Mau ake ouzilidwa . ( Luka 4 : 43 ) Yesu anadziŵa kuti Ufumuwo udzayeletsa dzina la Atate ake ndi kuthetselatu mavuto onse a anthu . Ngakhale kuti Adamu ndi Hava anafunikila kukhala ndi moyo kwamuyaya , io sanali ndi moyo wosafa . Ngati timaphunzila ndi anthu ena buku la Zimene Baibo Imaphunzitsa ndi buku la Cikondi ca Mulungu , nanga kuli bwanji kuphunzila ndi ana athu ? Kodi Mose anazindikila ciani pankhani ya ‘ zosangalatsa zaucimo ’ ? Tingaonetse bwanji kuti tikucita zinthu mogwilizana ndi kudzipeleka kwathu kwa Mulungu “ tsiku ndi tsiku ” ? ( Deuteronomo 30 : 19 , 20 ) Ngati Mulungu angakakamize anthu kutsatila njila ina yake , ndiye kuti akuwalanda ufulu wodzisankhila zocita . Kuwonjezela apo , unam’thandiza kucita zinthu zimene sakanatha kucita mwa mphamvu zake zokha . MBILI YANGA : N’NALI N’CIZOLOŴEZI COTAMBA ZAMALISECE ( Luka 12 : 4 ) Musakayikile ngakhale pang’ono kuti Yehova adzakuyang’anilani monga mmene analonjezela , ndi kukupatsani “ mphamvu yoposa yacibadwa , ” ndiponso adzakuthandizani kuti musagonje pamene muopsezedwa . — 2 Akor . Anthu ocokela ku Poland anali kugwila nchito mwakhama . Iwo anali kutsatilabe cikhalidwe ca kwao , ngakhale pankhani ya cipembedzo . Zimenezi zinathandiza kuti “ osankhidwawo , ” kapena kuti Akristu odzozedwa , athaŵe mumzindawo ndi m’madela ozungulila mzindawo . Kodi Yehova angakuthandizeni bwanji ? Anthu amaona kuti dayamondi ndiponso cuma n’zofunika kwambili . Kodi Aroma 8 : 21 iyenela kutithandiza kufunsa kuti ciani ? Pamene munali kukula , muyenela kuti munaona anthu ambili akubatizidwa . Kuonjezela apo , muziyamikila moyo umene muli nao . 1 : 25 ) Yehova , amene anapeleka lamulo langwilo limenelo amadziŵa bwino zimene anthu amafunikila kuti akhale na cimwemwe ceni - ceni . 1 , 2 . ( a ) N’cifukwa ciani simukaikila kuti Yehova amakonda anthu ake ? Liu la Cigiriki limene Paulo anaseŵenzetsa litanthauza “ kusumika maganizo na mtima wonse pa cinthu cinacake , ndi kuyesa kucipangila mapulani a mmene ungacicitile ngati zingatheke . ” Kalalikile za ine ndi mtima wonse . Iyeyo anali kuweluza ndi kumenya nkhondo mwacilungamo . Mgwilizano wao unali kuonekela pamene ‘ mafuko onse a Ya ’ anali kukumana kuti alambile Mulungu . Conco , n’kofunika kuti tizisamala ndi anthu amene timagwilizana nao masiku ano otsiliza . Ngati anthu sanalabadile uthenga wathu , tiyenela kuganizila zimene zawacititsa kuti asamvetsele . Matthew , amene amagwila nchito yokonza zinthu zoonongeka , anati : “ Anthu amaganiza kuti pamene ugwila nchito kwambili kuti upeze zofunikila pa umoyo , m’pamenenso umapeza zocepa . ” Abigayeli atamva zimenezi , anatenga zakudya ndi zakumwa ndi kupelekela Davide ndi anthu ake . Ndani makamaka amene afunika kuona kuti timawaganizila ? 13 Mbili Yanga ​ — Kukhala Wogontha Sikunanilepheletse Kuphunzitsa Ena Nthawi imeneyo , anthu anali kucita zoipa za mtundu uliwonse , ndipo anali kuzicita mwaukatswili . Kodi Yesu anaphwanya Lamulo mwa kuimilila pamwamba pa kacisi wopatulika ? Komabe , mphatsoyo inabweletsa udindo waukulu kwa iye . Ndinamulanda bukulo ndi kunena kuti , “ Ndangofika pakati pa bukuli , koma ndaona kale kuti ndidzakhala wa Mboni . ” Anayamba kukhala na m’bale wina amene ni mpainiya , anapeza nchito ya maola ocepa , ndipo anayamba upainiya . Jean - David , amene tam’chula kale , anati : “ Tinaona mzimu woceleza umene abale ali nawo . Ndipo n’zosangalatsa kuthandiza mpingo umene muli olengeza ufumu ocepa . ” Mbali yaikulu ya osamalila wodwala ni kupeleka citonthozo . Musaiŵale kuti Mulungu amaticenjeza kuti tisamacite zamizimu kapena zamatsenga . — Deuteronomo 18 : 10 - 12 ; Yesaya 1 : 13 . Kodi Yesu analemekezedwa bwanji pa nthawi ya kubadwa kwake komanso pamene anapita naye ku kacisi pambuyo pa masiku 40 ? Zimene zinanidabwitsa n’zakuti mnyamatayo anabwela pafupi n’kuniuza kuti : “ Unikhululukile cifukwa ca zimene n’nakucitila dzulo usiku . “ Mudzakhala Mboni Zanga , ” 7 / 15 Ambili amene amacezela okalamba kaŵili - kaŵili amati : “ Ndinapita kukacezela wokalamba wina , ndipo anandilimbikitsa kwambili . ” — Miy . Pa zaka zonsezo , Yehova anaona mavuto onse amene mtumiki wake anali kukumana nao . ( 1 Atesalonika 2 : 13 ) Timasangalalabe ndi madalitso a Yehova ngakhale kuti Satana amatizonda ndi kutitsutsa . — 2 Akorinto 4 : 4 . Akhiristu amene ali na mavuto aakulu m’banja afunika kupempha thandizo kwa akulu . Anthu ambili odwala ndiponso olemala anali kupita ku dziwe la Betesida . Pambuyo pake , ambili a io analapa ndipo anakhalanso paubale ndi Atate wathu wacifundo wakumwamba . ( Sal . Ine na Livija takhala na mwayi wotumikila limodzi pa Beteli kwa zaka zoposa 40 . M’nkhani yotsatila , tidzakambilana mmene tingaseŵenzetsele mwanzelu ufulu umene tili nawo , kuti tipitilize kulemekeza Yehova , Mulungu wa ufulu weni - weni mpaka muyaya . [ Mau okopa papeji 5 ] “ Ifetu timamudalila kuti ciliconse cimene tingamupemphe mogwilizana ndi cifunilo cake , amatimvela . ” — 1 Yohane 5 : 14 [ Mau okopa papeji 6 ] Pamene anali kukula , Yehova anali nao . Koma kumeneko , anali osatetezeka . 17 : 11 ) Panthawiyo , kudelalo kunalibe mpingo . Conco , alongo aŵili aja anali kucititsa misonkhano m’nyumba ya banja lina lacidwi , ndipo opezekapo anali ocepa . Mungayambe mwa kumuonetsa mmene angakonzekelele zimene mumaphunzila naye . Ngati munthu wacita cidwi , iye amayang’ana kacizindikilo kena kamene kamacititsa kompyutayo kukamba kuti , “ Kodi mufuna ndiziphunzila nanu Baibulo ? ” Tingaonetse bwanji kuti tili na cikondi ceni - ceni ? Amene amakonda mkazi wake amadzikonda yekha . ” Inunso angakuthandizeni mmene anathandizila atumwi ake . 1 / 1 Koma kuti mwayi umenewu usakatiphonye , tifunika kuikabe maso athu pa Yehova na kumumvela nthawi zonse . ( 1 Yoh . Ndinaona kuti cili bwino kucoka kuti ndizikagwila nchito yothandiza banja langa m’malo molemeletsa anthu ena . 11 : 32 - 34 . Pa nthawiyi Lameki anali wamng’ono , ndipo n’kutheka kuti anacita cidwi ndi kulimba mtima kwa Inoki , ambuye ake . 3 Mmene Amuna Anayi Okwela pa Mahosi Amakukhudzilani Mukapanga lamulo kapena cosankha , muzipeza nthawi yoyenelela yofotokozela ana anu acinyamata cifukwa cake mwacita zimenezo . Kodi cikhulupililo ca Mkhristu cingayesedwe bwanji ? ( Miy . 23 : 23 ) Yesu anakamba kuti timafunikila “ mau onse otuluka pakamwa pa Yehova . ” ( Mat . ( Yeremiya 35 : 1 - 19 ; 39 : 15 - 18 ; 45 : 1 - 5 ) Cizindikilo cimene anaikidwa cinali cophiphilitsa , ndipo cinali kutanthauza cabe kuti adzapulumuka . 1 FUNSO : Kodi Mulungu n’ndani ? Ngati zinali conco , tingamvetsetse cifukwa cake . Akafika kumsonkhano , ambili anali kukhala na Mboni za m’delalo , zimene zinali kuwalandila mwacikondi m’nyumba zawo . Kodi pangakhale njila yothetsela nkhanza imeneyi ? Kuwonjezela apo , ubwenzi wathu ndi Mulungu walimba kwambili , ndipo ndife ogwilizana kwambili pabanja pathu . ” Tinali kukhulupilila kuti pa cifukwa cimeneci , Yehova analola Babulo Wamkulu kutengela anthu Ake mu ukapolo kwa kanthawi . Mfundo za coonadi ca m’Baibulo zinasintha umoyo wanga kukhala wabwino . “ Uthenga wabwino uwu wa Ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi kumene kuli anthu , kuti ukhale umboni ku mitundu yonse , kenako mapeto adzafika . ” — Mateyu 24 : 14 . AKHIRISTU oona ali na ciyembekezo cabwino maningi . Sitiyembekezela kuti Yesu kapena Atate wake angaticitile cozizwitsa ngati cimeneci masiku ano . KUYAMBILA pa Abele , munthu woyamba wokhulupilika , alambili a Mulungu akhala akulimbana ndi mayeselo . Malinga ndi zimene zinalembedwa pa Salimo 15 , Davide anaimba nyimbo yofotokoza zimene tifunika kucita kuti ‘ tikhale mlendo m’cihema ’ ca Yehova kapena kuti tikhale pa ubwenzi ndi Mulungu . ( Sal . Kodi inuyo mumazigwilitsila nchito ? Atumiki a Mulungu amakono angaphunzilepo kanthu pa zitsanzo za m’Baibulo zimenezo . Eliezere anapempha Mulungu kumutsimikizila kuti mkazi amene afuna kuti Isaki akakwatile akamupeze ku citsime . Pofotokoza lemba la Mlaliki 9 : 10 iye anati : “ ‘ Ciliconse cimene dzanja lako lapeza kuti licite , ucicite ndi mphamvu zako zonse . ’ M’tauni ina ya anthu 150 , ku United States , anthu 400 anapenyelela seŵelo pasukulu ina panthawi zosiyanasiyana . Cisautso cacikulu cikadzatsala pang’ono kuyamba , Mulungu adzadinda cidindo comaliza odzozedwa a khama amene adzakhala akali padziko lapansi . ( Chiv . Iye anatumiza Mwana wake , Yesu , padziko kuti apeleke moyo wake kukhala dipo la macimo athu . Kodi mungamve bwanji ? Mwacionekele , mungakhale ndi nkhawa , mungacite mantha , ndipo mungadzione kuti ndinu wosayenelela . Ndi malo okhalamo otani amene Yehova anatipatsa ? ( Maliko 13 : 10 ) Buku lina lofotokoza za cipembedzo linakamba kuti cinthu cofunika kwambili kwa Mboni za Yehova ndi nchito yolalikila . Ana ambili amakhala opusa kapena kukhala osamvela ngati makolo ao amawacitila zilizonse zimene akufuna ; koma si mmene Yosefe analili , iye anaphunzila makhalidwe abwino ambili kwa makolo ake ndipo anali wolimba m’cikhulupililo ndiponso anali kusiyanitsa cabwino ndi coipa . Tingawalimbikitse mwa kuwauza kuti timawakonda kwambili . 12 : 18 ) N’zoonekelatu kuti kunyada kumasokoneza mtendele mumpingo . Mutu wa nkhani umenewu unakhumudwitsa ena cifukwa m’nthano ya ku Korea , Shim Cheong ndi mtsikana wokondedwa amene wodzipeleka pa kuthandiza atate ake osaona . Robison ) , Feb . Tiwayamikila kwambili anchito odzipeleka amenewa pogwila nchito imeneyi molimbika . 119 : 165 ; Yes . 54 : 13 ) Ngati tiyesetsa kukhala mwamtendele na ena , timaonetsa kuti timawakonda kwambili , ndipo zimenezi zimakondweletsa Atate wathu wakumwamba . — Sal . N’cifukwa cakuti nkhaniyi ikhudza anthu onse kuphatikizapo angelo . ( Luka 2 : 36 , 37 ) Pamene wansembe anali kufukiza nsembe usana ndi usiku m’kacisi , Anna anali kukhala pakati pa khamu la anthu amene anali kusonkhana m’bwalo la kacisi . ( Mlaliki 4 : 1 ; 8 : 9 ) Koma Mulungu Wamphamvuyonse walonjeza kuti adzabweletsa boma limene lidzaphwanya maboma onse ndi kuyamba kulamulila . Enanso amene amafunikila cilimbikitso ni abale na alongo amene sali pa banja cifukwa cofuna kumvela lamulo lakuti tiyenela kukwatila kokha “ mwa Ambuye . ” ( 1 Akor . N’nali wokonzeka kugwila nchito iliyonse imene yapezeka , ndipo tinayamba kupewa kugula zinthu zosafunika kweni - kweni . Ana opanduka ( Onani palagilafu 16 ) Kodi n’ciani cingatilepheletse kuikabe maso athu pa Yehova ? M’malomwake , muli dzina la udindo lakuti “ Ambuye ” kapena dzina la mulungu wa kumaloko . Conco , kuti Yehova akatiteteze pa cisautso cacikulu , tifunika kudziŵa kuti iye ali ndi anthu ake padziko lapansi , ndipo anthuwo ali m’mipingo . Ndipo tidzapindula bwanji tikacita zimenezo ? Monga Atate wacikondi , iye anateteza ndi kusamalila anthu ake okhulupilika monga Nowa , Abulahamu ndi Davide . NYIMBO : 112 , 89 ( a ) N’cifukwa ciani Ufumu wa Mulungu wokha ndiwo ungacotsepo mavuto a anthu ? Koma mu 1993 , gulu la ofufuza zinthu zakale linafukula mwala wakale kwambili , ndipo pamwalapo panali liu limene limatanthauza kuti “ Nyumba ya Davide . ” Mwacitsanzo , pa Mateyu 5 : 44 pali uphungu wa Yesu wonena kuti : “ Pitilizani kukonda adani anu ndi kupemphelela amene akukuzunzani . ” sakondwela na munthu amene amanyalanyaza nchito yake ? Iye anakambanso kuti ngakhale kuti a Mboni anazunzidwa kwambili , anakhalabe “ odalilika ndi odekha , ” ndiponso anaonetsa kuti anali “ okhulupilika ndi ogwilizana . ” Ana a Mulungu onse a kumwamba ndi a padziko lapansi adzagwilizana ndi Atate wao wa kumwamba monga banja limodzi . Tizikumbukila kuti aliyense amene amatamanda dzina la Yehova ndi wamtengo wapatali kwa iye . Malangizo amenewa ni ocokela kwa Mulungu amene amatiuza maganizo ake kudzela m’Mau ake olembedwa . ” Koma ine , lemba limene linanilimbikitsa kwambili ni Salimo 55 : 22 . Kodi kukhulupilila kuti Kristu anauka kumatikhudza bwanji ? Ngati timakonda coonadi monga mmene wamalonda anakondela ngale ija , tidzakhala okonzeka kusiya zilizonse n’colinga cakuti tikhale nzika za Ufumu wa Mulungu , ndi kupitiliza kucita zinthu monga nzika . Kodi Yehova anadalitsa bwanji atumiki ake akale ? Nanga masiku ano ? Kodi n’kulakwa Mkhiristu kulila malilo na kumva cisoni cifukwa amakhulupilila kuti akufa adzauka ? Ndiyeno , khungu linabwela pamwamba pa mnofu . Mlongo wina wa zaka za m’ma 80 , dzina lake Christa anadandaula kuti : “ Cimaŵaŵa kwambili ukamalephela kucita zambili mu utumiki monga mmene unali kucitila kale . ” Kodi Mumalola Kuti Woumba Wamkulu Akuumbeni ? N’ciani cinganithandize kuthetsa mantha kuti niziimba mokweza na mokondwela ? Izi sizinathetse cikhumbo cathu cokatumikila pa Beteli , koma panatenga nthawi yaitali kuti tipeze mwayi wa utumiki umenewu . ( Miy . 23 : 26 ) Ngati tili m’banja limene ena si Mboni , kodi timapempha Yehova kuti atithandize kukhalabe na khalidwe labwino olo kuti amene tikhala nawo alibe khalidwe labwino ? Pierce ) , 12 / 15 12 : 40 - 42 ) “ Zaka 430 ” zinayamba pamene pangano la Yehova ndi Abulahamu linakwanilitsika mu 1943 B.C.E . Ndipo iye anaonetsa kudzicepetsa pamene mtumwi Paulo anamudzudzula pamaso pa anthu . 17 : 22 ) Ndithudi , ngati mukulitsa cimwemwe canu , mungathe kukhala na thanzi labwino . Kodi Akristu ayenela kuona motani ciyembekezo cao copatsidwa ndi Mulungu ? Anthu ambili analandila kapepalako ndipo analimbikitsidwa ndi zimene anaŵelenga . Conco , tiyenela kukhala okonzeka kuvutikila abale ndi alongo athu ngakhale kuwafela kumene . — 1 Atesalonika 2 : 8 . Kodi Yesu anaonetsa bwanji kuti mkazi wamasiye anali wamtengo wapatali kwa Mulungu ? Khalani odekha makamaka pamene io akuphunzila cinenelo ndi cikhalidwe canu . M’kupita kwa nthawi , mu 1914 , anatulutsa “ Sewero la Pakanema la Chilengedwe , ” ndipo mu 1917 anatulutsa buku lochedwa The Finished Mystery . Kodi nidzakwanitsa kudzisamalila ? Yesu yekha ndi amene akanatha kucita zimenezi . ( a ) Kodi cikwati cimakhudzidwa bwanji ngati okwatilana akhala motalikilana ? Pofuna kumukopa , io anati : “ Mphunzitsi , tikudziŵa kuti inu mumanena zoona ndipo mumaphunzitsa njila ya Mulungu m’coonadi . ” Anthu Acigiriki amene anabwela ku Yerusalemu kudzacita cikondwelelo ca Pasika , anaona zimene Yesu anacita cakuti anacita cidwi kwambili . Dzifunseni kuti : ‘ Kodi nthawi zina nimalola thupi langa kapena maganizo anga kunitsogolela ku zinthu zosayenela ? NYIMBO : 110 , 2 M’kupita kwa nthawi , tinakhala na cimene Yesu anacicha “ mosungilamo cuma , ” cimene ndi mfundo za coonadi , zakale ndi zatsopano . Malemba amakambanso kuti : “ Amuna akonde akazi awo monga matupi awo . ‘ Nanga zinthu zidzakhala bwanji adzukulu anga akakula ? ’ Maurizio anafotokoza kuti : “ Pa nthawi ina , n’nacita zolakwa zazikulu zimene zinacititsa kuti ine na mnzanga tisamagwilizanenso . ” NYIMBO : 37 , 116 3 : 16 ) Motelo , Kristu adzakhala “ Atate Wosatha ” kwa io . — Yes . 1 : 10 - 12 . 1 : 2 ; Aheb . Patapita nthawi , Daniel anasintha ndipo anayambanso kutumikila pa maudindo ake mumpingo ali ndi cikumbumtima cabwino . N’zifukwa ziti zimene anachula ? 19 : 11 . Patrick ndi Hannah analalikilanso ku Angaur , kacilumba kakang’ono kamene kali ndi anthu 320 . Kodi dipo imatimasula bwanji ? N’zacisoni kuti Kaini anapha m’bale wake , ndipo anakhala woyamba kupha munthu . — Gen . Nkhondo Imene Inasintha Zinthu Padziko 3 Mwacitsanzo , Nsanja ya Mlonda yogaŵila ndi nkhani zimene zimapezeka pa jw.org zimafotokoza Baibulo pogwilitsila nchito mau osavuta kumvetsa . Kaya takhala nthawi yaitali m’coonadi kapena ai , tifunika kuuzako ena za gulu la Yehova . Timaona mmene mzimu wake woyela umatithandizila kugwila bwino nchito yolalikila uthenga wabwino . N’cifukwa ciani Mulungu amagwilitsila nchito mau osavuta akamakamba ndi anthu ? Ndinakondwela kwambili kuti anandigwilitsila nchito . ” * Kuwonjezela apo , tuzipangizo tumenetu tumacititsa kuti madzi a pa khomo la cibalilo akhale otikama kwambili , ndipo izi zimalepheletsa mbeu ya mwamuna kuloŵa m’cibalilo . Mboni za Yehova zikulalikila uthenga wabwino wa Ufumu padziko lonse lapansi Ali m’ndende anakamba ndi Mboni za Yehova ndipo anayamba kuphunzila Baibulo . * Koma kodi atate ake osakhulupilila anamvela bwanji pamene mwana wao anasankha kukhala mtumiki woyendayenda wacikristu ? Pamene tiŵelenga macaputa aŵili oyambilila a Genesis , timaona kuti Adamu na Hava anali na ufulu weni - weni umene anthu masiku ano amaulakalaka . Panalibe cowayofya , sanali kusoŵa ciliconse , ndiponso panalibe amene anali kuwapondeleza . Ena amalandila cisamalilo ca Boma koma ena samatelo . Ndipo ena anali kulimbikitsa ciphunzitso cakuti kucitako zosangulutsa paumoyo ndi kulakwa . Mlongo wina anafotokoza mmene mau a M’bale Charles T . N’nali kudwala - dwalanso maleliya , matenda a amoeba , na njoka za m’mimba . 3 : 8 - 10 . Kodi Malemba amaonetsa bwanji kuti cikondi n’cofunika ? Yesu anakamba kuti tizikonda Mulungu ndi munthu mnzathu . Yehova amaona mmene mtima wathu ulili . Amadziŵa zimene timaganiza ndi kulakalaka ndipo sitingamubise kalikonse . Anali kulila nane pamodzi , kunitonthoza , ndi kunipangitsa kudzimva kuti ndine wofunika . Ndi funso liti limene tingafunse ponena za makambilano a pakati pa anamwali anzelu ndi anamwali opusa ? Kudziŵa bwino zamtsogolo kudzakuthandizani kukhala okonzeka . Koma cifukwa ca kampeniyi , citsanzo ca abale a kumeneko , ndi mapemphelo , n’nakwanitsa kucita zimene kale n’nali kulephela . Anakhala munthu wosauka kwambili ndi wovutika . Kukamba zoona , zimatsitsimula ngati aliyense wa ife acitako mbali yake kuti ‘ tizilimbikitsana . ’ — Aroma 1 : 11 , 12 . Nthawi ina , mosadziwa tinafika pa mudzi wina ndipo tinapeza kuti akucita msonkhano wandale . Lekani akuuzeni yekha zina zokhudza umoyo wake : ▪ Phunzitsani Ana Anu Kutumikila Yehova Koma nafenso tifunika kucitapo kathu kuti tithetse mavuto amene tingathe , ndi kuthandiza ena . Patapita zaka zoposa 60 Yesu atafa , Yohane amene Yesu anali kumukonda anaona masomphenya a Yesu . Komabe , asainimenti yotsatila inathetsa vuto limeneli . Mwacitsanzo , Hava anali kuvutika kwambili ndi pakati , komanso popapa . Ni mmenenso zinakhalila kwa akazi onse . Pa nthawi ina , nayenso mtumwi Paulo anafotokoza Malemba mwanjila imeneyi pokamba na Ayuda a mu mzinda wa Antiokeya wa ku Pisidiya . ( b ) Ndi zinthu ziti zimene tiyenela kupewa malinga ndi cenjezo la pa Miyambo 7 ? Kodi anthu othaŵa kwawo ( a ) tingawathandize bwanji mwauzimu ? Kodi anatengela amayi ake , amene anali Muamoni ? ( 1 Maf . Cifukwa ca nsanje , abale ake anam’gulitsa monga kapolo . Simuyenela kukhala okhutila ndi zinthu zokha zimene munaphunzila musanabatizidwe . Panthawiyo mwana wa John anali ndi zaka zitatu cabe . Pamene makhalidwe akuipilaipila m’dziko la Satanali , Yehova amakondwela kwambili kuona atumiki ake odzipeleka akuyesetsa kupewa maganizo oipa ndi kutsatila mfundo zake za makhalidwe abwino . ( Gen . 4 : 6 , 7 ) Mwanjila ina , tingakambe kuti Yehova anali kuuza Kaini kuti : “ Ukalapa na kukhalabe ku mbali yanga , na ine nidzakhala ku mbali yako . ” Tisakhale monga anthu a m’nthawi ya atumwi amene sanali kucita zimene anali kuphunzitsa . Mu April 1951 , olamulila anayamba kutenga mwacikakamizo Mboni za kum’madzulo kwa dziko la USSR n’kukaziika ku Siberia . Ngati munakukila mu mpingo wina , n’kutheka kuti inunso muli na mantha . Kusamba kumene ana a Aroni anali kucita kumaimila kuyeletsedwa kwa aja amene anasankhidwa kukakhala ansembe a kumwamba . Vesi imeneyi imati : “ Poona cikhamu ca anthu , [ Yesu ] anawamvela cisoni , cifukwa anali onyukanyuka ndi otayika ngati nkhosa zopanda m’busa . ” Kuonjezela pa mabuku , gulu la Yehova limakonzanso maautilaini a nkhani ogwilitsila nchito pamisonkhano ya mpingo , yadela , ndi yacigawo . Ngakhale kuti Yehova amapeleka malangizo ake kwa onse , iye sakakamiza munthu kuwatsatila . Yudasi amene anam’peleka anacita kum’psompsona monga “ cizindikilo cimene anagwilizana , ” kuti gulu la anthu limuzindikile Yesu . — Maliko 14 : 44 , 45 . 1 , 2 . ( a ) Kodi alendo ambili amakumana na mavuto yabwanji masiku ano ? N’ciani cimene tiyenela kukumbukila munthu wina akatipatsa malangizo okhudza thanzi ? Satana anatenga Yesu mwacindunji ndi kupita naye ku kacisi ? “ OFALITSA Ufumu ku Britain — Galamukani ! ! ” NYIMBO : 63 , 129 Tiyenela kudziŵa ciani ponena za Yehova ? 3 : 1 - 5 ) Cinanso , timayeletsa dzina la Mulungu mwa kuyesetsa kuthandiza anthu a m’gawo lathu kuona kuti Yehova ni woyenelela “ kulandila ulemelelo ndi ulemu ” ndi mphamvu . ( Chiv . ( Gen . 41 : 1 , 37 - 43 ) Pamene Yosefe anabala ana aŵili amuna , “ mwana woyambayo . . . anamucha dzina lakuti Manase , cifukwa anati , ‘ Mulungu wandiiŵalitsa mavuto anga onse , ndi nyumba yonse ya bambo anga . ’ Caka catha , tinapulinta makope a tumapepa tumenetu okwana 440,000,000 m’zinenelo zoposa 530 . Sindinali kufuna kuphunzila Baibulo ndi Mboni , koma ndinali kukonda kupita ku misonkhano yao . Sitikukaikila kuti mumatelo . Mulungu sadzalola zoipa kukhalaponso . Afarao akale a ku Iguputo anayesetsa kwambili kufuna - funa njila yakuti azikhala ndi moyo wosafa . ( 2 Timoteyo 3 : 16 ) Iwo amalemekezanso dzina la Mulungu . Pamene anali wacinyamata , Mfumu Solomo anali kutsatila malamulo a Yehova . ( b ) Kodi kukhulupilila Yehova panthawi ya mavuto kumalimbitsa bwanji ubwenzi wathu ndi iye ? “ Komabe , Kristu anaukitsidwa kwa akufa , n’kukhala cipatso coyambilila ca amene akugona mu imfa . Poyankha , Yesu anakamba fanizo la Msamariya amene anasamalila mokoma mtima Myuda wa paulendo amene anamenyedwa ndi acifwamba . Koma atakana kugona ndi mkazi wa abwana ake , iye anapatsidwa mlandu wabodza wakuti anafuna kugwilila mkazi wa abwana ake . Kodi anthu amene afunikila thandizo mu utumiki tingawathandize bwanji ? Ngati tiyesetsa kumumvela , kumudalila , na kukhala odzicepetsa , iye adzationa kuti ndise amtengo wapatali . — Hag . Iye anati : “ Ndinali kufuna kulaŵa ‘ ufulu ’ umene dziko limapeleka . ” Conco , kuti tipindule ndi kukoma mtima kosatha kwa Yehova ndi kupewa mkwiyo wake , tifunika kudana ndi zimene iye amadana nazo . ( Sal . Tinali kukonzekelatu nkhani zokakamba nawo poceza kuti maceza athu akayende bwino . Kutsatila ziphunzitso za Yesu monga ophunzila ake , kudzatithandiza kukhala na umoyo wacimwemwe na wokhutilitsa . ( 2 Tim . 4 : 17 ) Monga Paulo , nafenso pamene tiika nchito yolalikila patsogolo mu umoyo wathu , tiyenela kukhulupilila kuti Yehova adzaonetsetsa kuti zonse zimene timafuna ‘ zawonjezedwa kwa ife . ’ ( Mat . Kodi mungathandize bwanji mpingo kukhala wogwilizana ? Onani Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 , tsamba 13 - 14 , ndime 14 - 18 . Ngati ungodziŵa cabe ziphunzitso zoyambilila za m’Baibulo , sungakhale na cikhulupililo colimba kweni - kweni . Mwacionekele , simungagwile nchitoyo kwa nthawi yaitali , mungafooke n’kuisiya . Ndi zitsanzo ziti zimene zikuonetsa kuti panopa tingathe kufotokoza mafanizo a Yesu momveka bwino ? 18 : 1 - 3 , 13 ) Koma pambuyo pake , Senakeribu anabwela kuti awononge Yerusalemu . Kodi Davide anacita bwanji ? — 1 Mbiri 17 : 1 - 4 , 8 , 11 , 12 ; 29 : 1 . Makolo ena amaona kuti ni bwino kuti mwana wawo acedweko kubatizika n’colinga cakuti aciteko maphunzilo apamwamba coyamba na kupeza nchito yabwino . Pocita izi , iwo angakhale na colinga cabwino ndithu . [ Mau apansi ] Liu la Cigiriki limene linatembenuzidwa kuti “ manda ” limatanthauza “ malo ogonako . ” Komabe , kukambilana umboni wakuti ciyembekezo cimeneci n’codalilika kungalimbikitse kwambili cikhulupililo cathu . ( 1 Maf . 21 : 27 - 29 ) Yehova , amene “ amayesa mitima , ” anamucitila cifundo Ahabu . — Miy . Kodi ufulu wanu wosankha mukuuseŵenzetsa popititsa patsogolo nchito ya Ufumu kapena zofuna zanu ? Tingaonetse Bwanji Kuti Timakonda Yehova ? Ndiyeno m’bale wokhumudwayo anakamba kuti , “ Mwakamba zoona . ” Koma kodi Yehova anadabwa ? Ŵelengani Aefeso 6 : 16 . Titamufotokozelanso zimenezi , mkulu wa asilikaliyo anatiuza kuti , “ Cabwino , mutenge hachi kuti muzinyamula asilikali amene avulala pa nkhondo n’kuwapeleka kucipatala . ” A Zulu : A Zimba , kunena zoona , ndimakondwela kukambilana nanu za m’Baibulo kumene timakhala nako nthawi zonse . Mwina ena a inu mukupilila matenda kapena zoofoka zaukalamba , ngakhalenso kusungulumwa . Tiyeni tikambilane zitsanzo izi : ( Onani bokosi lakuti “ Zimene Zingatithandize Kupeleka Yankho . ” ) Popeza Yehova ni Mulungu wacifundo , nafenso mwacibadwa timafunila anzathu zabwino . Monga kholo , kukhala wozindikila n’kofunika kuti muteteze ana anu kuti asacite ciliconse cimene cingakhumudwitse Yehova . Mame ndi dalitso locokela kwa Yehova . Apa lomba kumasuka ku cipembedzo conama kunali pafupi . Mwa ici , n’naganiza zoyambanso kutumikila Yehova na mtima wanga wonse . ” ( a ) Mungadziŵe bwanji mmene ana anu amaonela utumiki ? NYIMBO : 38 , 56 Mu 1952 , wapolisi anauza Maria kuti : “ Siya cikhulupililo cako , apo ayi ukapika ndende kwa zaka 10 . N’nabatizika mu 1941 nili na zaka 12 . Mwacitsanzo , abale na alongo athu ambili ali m’ndende ku Eritrea , Singapore , ndi South Korea , cifukwa amamvela mau a Yesu akuti osagwila lupanga . ( Mat . Koma kodi n’zoona kuti nthawi payokha ingathetse cisoni ? 6 : 10 ) Ndipo iye adzationetsa kukoma mtima kwake , mwina ngakhale m’njila imene sitinali kuyembekezela . 21 : 9 ; Yoh . 14 : 2 , 3 . Yobu sanadziŵe kumene mavuto ake anali kucokela , cifukwa cake mavuto anamugwela kapena cimene Mulungu analolela kuti mavutowo amucitikile . 7 ) Munthu wina dzina lake Diotirefe , anali ‘ kunenela zamwano ’ mtumwi Yohane ndi Akhristu ena . ( 2 Maf . 10 : 15 , 16 ) Ma Yehu Aakulu atatu amenewo , kapena kuti makalavani anali a mamita 2.2 m’litali , 1.9 m’lifupi , ndi 1.9 kutalika kwake , ndipo kalavani lililonse munali kugona apainiya 6 . Nanga bwanji za Msulami ? 2 : 13 , 14 ) Panthawi ina Mose anafunsa Yehova kuti : “ Nanga Farao akandimvela bwanji ? ” 13 : 2 . Anthu ena amayamba kunyada na kudzikweza cifukwa ca kukongola , kuchuka , maluso a kuimba , mphamvu , kapena udindo umene ali nawo . N’ciani cimene akulu ayenela kucita kuti adziŵe ngati munthu ni wolapadi ? Patsiku limeneli , Yehova , kupyolela mwa mzimu wake , anakhazikitsa mtundu watsopano , umene ndi Isiraeli wa kuuzimu , kapena kuti “ Isiraeli wa Mulungu . ” Posapita nthawi , iye anatenga zovala zake zonse n’kupita osandilaila ndipo anandisiya ndi ana aŵili . ” Kodi mabwenzi athu apamtima ayenela kukhala anthu otani ? N’ciani cingatithandize kupilila mavuto aliwonse amene tingakumane nawo ? A Yohane : Zoona ? Yesu anauza otsatila ake kuti : “ Kapolo sali wamkulu kuposa mbuye wake . Maka - maka pamene ticita na vuto kapena nkhani imene tinaizoloŵela , tifunika kusamala kuti tisadalile nzelu zathu . Makhalidwe amenewa amamuthandiza kupilila mavuto aakulu popanda kukhumudwa . Yehova anali kufuna kuti iwo akhale odzipeleka kwa iye yekha ndi kuti azimukonda ndi mtima wawo wonse , moyo wawo wonse , ndi mphamvu zawo zonse . Olo kuti poyamba Adamu na Hava anali na ufulu m’njila zambili , Mulungu anawaikila malile kapena kuti malamulo . M’nthawi zakale , woumba mbiya anali kucotsa miyala ndi zinthu zina zosafunika mu dothi asanayambe kuumba . Pokhala na cikhulupililo conse kuti Yehova adzadalitsa khama lawo , iwo anali ofunitsitsa kucita zonse zimene akanakwanitsa . Koma kucita zimenezi kunali kovuta . Iye anafunika kulimbitsanso cikondi m’banja lake . Kuonjezela pa miseu imeneyi , Aroma analinso kugwilitsila nchito zombo zambili . Iwo anali kuyenda pamitsinje ikuluikulu ndiponso panyanja kuti afike ku madoko onse mu ufumuwo . Koma tiyenela kusamala kuti tisayambe kukonda kwambili ndalama , kapena kufuna nchito yapamwamba . 58 : 11 . Ena mwa mapindu amenewo ni awa : napeza mabwenzi eni - eni , umoyo wopindulitsa , komanso cimwemwe ceni - ceni . 15 , 16 . ( a ) N’cifukwa ciani kuika maganizo athu pa zinthu zakumwamba n’kofunika ? “ Koma nzelu zimakhala ndi anthu odzicepetsa . ” — MIY . Yesu anawayankha kuti : “ Anthu abwinobwino safuna dokotala , koma odwala ndi amene amamufuna . Angaphunzilenso kukhala woganizila ena . “ Ngati ana aphunzitsidwa kuganizila ena m’banja , ku sukulu , komanso m’dela lawo , amakhala ofunitsitsa kucitila ena zinthu mokoma mtima . ” Imakamba conco buku yakuti , Parenting Without Borders . Cifukwa pang’onopang’ono zimenezi zingaononge ubwenzi wathu ndi Yehova . N’ciani cimene cingatilepheletse kupitiliza kuyang’ana kwa Yehova ? Ndipo zimene tinaphunzila m’Baibulo zinapangitsa banja lathu kukhala logwilizana kwambili . ” — Eziquiel . DZIKO : GERMANY 28 : 7 . Yesetsani kuona zimene amakonda , cifukwa zimene munthu amakonda zimakhudza zimene amalakalaka . Timamva ngati Chantel wa ku France amene anati : “ Mlengi wa zinthu zonse , Wamphamvuyonse m’cilengedwe , Mulungu wacimwemwe , wandiuza kuti : ‘ Pita ! Baibo imatilimbikitsa kuti : “ Yandikilani Mulungu , ndipo iyenso adzakuyandikilani . ” — Yakobo 4 : 8 . ( b ) Nanga tungakuthandizeni bwanji kukonzekela maulendo obwelelako ? Akulu akamayesetsa kuthandiza ena , pamakhala abale ambili amene angathandize mpingo kukhala wolimba ndi wogwilizana masiku ano ndiponso makamaka panthawi yovuta ya cisautso cacikulu . ( Ezek . Mogwilizana na mfundo imeneyi , lemba la Salimo 106 : 32 , 33 limati : “ Iwo anaputa mkwiyo [ wa Mulungu ] pa madzi a ku Meriba , moti Mose sizinamuyendele bwino cifukwa ca anthu amenewa . 1 , 2 . ( a ) Kodi kukhala mboni kumatanthauza ciani ? Nanga amtolankhani a dziko alephela m’njila ziti ? Tsopano , Sara anaona kuti inali nthawi youza Abulahamu za pulani imene anali kuganizila kwa nthawi yaitali . Iye anati : “ M’baleyo anakambilana nane kwa mamineti 15 pa nkhani ya zolinga zanga zauzimu . ” Kucita zimenezi kudzathandiza kuti azisangalala mu cikwati cao . Kuwonjezela apo , kaya ndife abale kapena alongo , tifunikabe kukhala ndi “ zocita zambili nthawi zonse mu nchito ya Ambuye . ” — 1 Akor . Iwo anafunikanso kupemphela mwamseli osati modzionetsela kwa anthu . M’Baibo , liwu lakuti lonjezo limatanthauza cowinda cimene munthu amapanga kwa Mulungu . ( b ) Nanga okalamba mumpingo angapemphe ciani kwa Mulungu ? Wosimba ni Douglas Guest Tikamaŵelenga Baibulo timamva za mavuto amene Zimiri anakumana nao cifukwa ca ciwelewele , ndiponso amene Gehazi anakumana nao cifukwa ca dyela . Kodi mau ndi zocita za Yesu zinaonetsa bwanji kuti ndi wodzicepetsa ? ( Ower . 2 : 3 , 11 - 23 ) Ganizilaninso zimene zinacitika panthawi ina , pamene anthu a Mulungu anafunika kupanga cosankha . 3 : 12 ; Yak . 2 : 15 , 16 ; ŵelengani 1 Yohane 3 : 17 . Popeza ndinalibe zocita zambili pakati pa nyanjapo , ndinagwilitsila nchito nthawi yanga yambili kuŵelenga Baibulo . Palinso mfundo ina yofunika kwambili imene ingatithandize kusankha zovala zoyenela — kuganizila cikumbumtima ca ena , kaya ca alambili anzathu kapena iyai . Koma palibe cimene nikanacita . MFUNDO YA M’BAIBO : “ Pitilizani kudziyesa kuti mudziwe kuti ndinu munthu wotani . ” — 2 Akorinto 13 : 5 . Lana atangomaliza pemphelo laciŵili munthu wina anamupatsa moni , amvekele “ Bwanji Lana ! Ukucita ciani kuno ? ” Ngati mwamuna na mkazi amamvela malamulo a Mulungu amakhala okondana , olemekezana , ndi acimwemwe . Kuti mudziŵe mmene anthu anakhudzidwila atalandila zofalitsa zathu , onani Nsanja ya Mlonda yacingelezi ya December 15 , 2000 , tsamba 32 ; August 1 , 1988 , tsamba 22 ; ndi Galamukani ! Kodi timatengela mwayi mipata yabwino imeneyo kuuza ena cifukwa cake timawakonda na kuwayamikila ? * Mwamsanga , tinayankha kuti “ Tidzapita ise ! ” N’zoona kuti m’magawo ena n’zovuta kupeza anthu ofuna kuphunzila za Mulungu . Kugwila nawo nchito yomanga imeneyi ni mbali ya utumiki wopatulika umene umalemekeza Mulungu , ndipo kungakuthandizeni kukhala wacimwemwe . Cifukwa aliyense ali na ufulu wosankha zimene afuna . Komabe , anthu ambili amakwatila na kubeleka ana olo kuti umoyo wa banja uli na zovuta zake . ( 1 Akor . Ngati timalola zotele kucitika , ndiye kuti tikuonetsa kuti sitiyamikila cifundo ca Mulungu ndi dipo lake . Tidzaphunzilanso zimene kukhala “ asodzi a anthu ” kumatanthauza . — Mateyu 4 : 19 . 12 : 9 , 12 , 17 ) Ngakhale kuti akupilila mayeselo aakulu , odzozedwa akupitilizabe kutsogolela nchito yolalikila . M’nthawi imeneyo “ mbewuzo zimamela ndi kukula . ” Asilikali aluso ayenela kuti anali kuponya miyalayi pa liwilo la makilomita 160 mpaka 240 pa ola . Mmene zinthu zilili paumoyo wathu zikhoza kukhudzanso mavalidwe athu . 3 : 8 . Mwacitsanzo , angapangitse munthu kudziona ngati wanzelu na wapamwamba kuposa anzake . Koma kodi iye angayambe kudzifunsa kuti , ‘ N’cifukwa ciani mwanayu wanipatsa duŵa limene n’langa kale ? ’ Danieli anati : “ Pa nthawi imeneyo Mikayeli [ Yesu Kristu ] , kalonga wamkulu amene waimilila [ kuyambila mu 1914 ] kuti athandize anthu a mtundu wako , adzaimilila [ pa Aramagedo ] . Kuti acotsemo mau ena acikale na kuikamo ena osavuta kumva . Koma anthu ambili amene amakhulupilila dipo , ali ndi mwai wokhala mabwenzi a Yehova . Mtsogolo io adzakhala ana a Mulungu , ndiponso adzakhala ndi moyo wosatha m’Paladaiso pano padziko lapansi . Nili pamwamba n’nadonsewa mwamphamvu na malaiti cakuti n’nakomoka . N’ciani cinathandiza Irina kupitiliza kutumikila Yehova mokhulupilika ? Tsiku lina , tinakumananso na zoopsa zina . Iweyo , magulu ako onse a asilikali , pamodzi ndi anthu ambili a mitundu ina , mudzaphimba dzikolo ngati mitambo . ” Taona umboni za zimenezi kwa anthu okhulupilika akale ndi amakono . Felisa : Patapita nthawi , ndinakwatiwa ndipo tinasamukila mumzinda wa Cantabria ku Spain . Anthu anali pafupi na ungwilo umene Adamu na Hava anataya . Mwacitsanzo , ponena za Yehova , lemba la Salimo 5 : 4 - 6 limati : “ Inu sindinu Mulungu wokondwela ndi zoipa . . . 13 : 4 , 7 . Ngati Yesu ndi Mulungu , n’cifukwa ciani anabwela pa dziko lapansi ndi kuphedwa ndi anthu ? ” Patapita miyezi yocepa , mkazi wa mlongosi wakeyo anamwalila . Madinaliwo anali malipilo a masiku aŵili . ( Mat . Masiku ano , Mboni za Yehova pa dziko lonse zimatengela Yesu mwa kuonetsa cikondi kwa anthu anzawo . ( Aroma 8 : 26 , 27 ) Kusinkha - sinkha mau olembedwa m’mabuku a m’Baibulo monga a Yobu , Masalimo ndi Miyambo , kudzatithandiza kuti tizitha kufotokoza za mumtima mwathu kwa Yehova . Iye anauza Eliya kuti : “ Nyamuka , pita ku Samariya ukakumane ndi Ahabu mfumu ya Isiraeli . ” Motelo anawo kunalibenso cifukwa cakuti anaphedwa . Zingatheke bwanji kukhala ndi banja lolimba ndi lacimwemwe ? Mofananamo , anthu amene adzapulumuka sadzaikidwa cizindikilo ceniceni . Mudzakondwela kutamba mavidiyo okamba za anthu azikhalidwe zosiyana - siyana amene apeza njila yopezela cimwemwe , ndipo ali na umoyo wacimwemwe . Conco , cimphepo citawomba , nyumbayo siinagwe . 10 : 20 . Ngakhale nditakalamba ndi kumela imvi , inu Mulungu musandisiye , kufikila nditanena za dzanja lanu lamphamvu ku m’badwo wotsatila , kufikila nditanena za mphamvu zanu kwa onse obwela m’tsogolo . ” — Sal . ( Yobu 2 : 3 - 5 ; Miyambo 27 : 11 ) Tikamayesetsa kuongolela zofooka zathu ngakhale kuti n’zovuta , timaonetsa kuti ndife okhulupilika kwa Yehova ndiponso kuti tifuna kuti iye azitilamulila . Mandy ananiuza kuti niŵelenge Danieli caputa 2 , ndipo n’nadabwa na zimene n’naŵelenga . Umboni wa zimenezi ni mau a pa Maliko 15 : 43 . Lembali limati : “ [ Yosefe ] anapita kwa Pilato molimba mtima kukapempha mtembo wa Yesu . ” Yelekezelani kuti mwaona combo cimene cikumila . “ Atate ndi wamkulu kuposa ine . ” — Yohane 14 : 28 . Ndipo sitikanapeza mayankho okhutilitsa a mafunso okhudza Mulungu , moyo , na tsogolo la anthu . Anthu ambili angayankhe kuti , “ ndi Mboni za Yehova . ” Patapita caka cimodzi ndi hafu , mai wina anatsegula citseko . Mulungu amaona kuti moyo ndi magazi n’zopatulika , ndipo adzalanga aliyense amene amazigwilitsila nchito molakwika . — Genesis 9 : 5 , 6 . Kodi tingayembekezele ciani m’tsogolo ngati titumikila Yehova na moyo wathu wonse ? Zaka zambili m’mbuyomo , Tony akayang’ana pa windo ali ku sukulu , anali kuona José ndi Rose ayenda mu ulaliki . Ngati mavuto aakulu apitiliza m’cikwati , mmodzi kapena onse aŵili angaganize zopatukana kapena kusudzulana . ( Ekisodo 16 : 31 ; Yoswa 13 : 2 ; 2 Samueli 3 : 31 ; Luka 15 : 9 ) Zinthu zimenezi zingakhale zosamvetsetseka kwa inu . Kapena pali kugwilizana kotani pakati pa kuwala ndi mdima ? ” “ Mudzakhala ufumu wanga wa ansembe ndi mtundu wanga woyela . ” — EKS . Palibe msinkhu woikika umene munthu afunika kufikapo kuti abatizike . Aphunzitsi a Baibulo anali “ kuŵelenga bukulo [ lopatulika ] mokweza . ” Yehova amaona moyo , maka - maka wa munthu , kukhala wopatulika . Komabe , mukhoza kuyamikila ngako Baibo yanu ya Malemba Oyela mukaphunzilako zina zake zokhudza Elias Hutter , katswili amene anakhalako zaka za m’ma 1500 . Iye anafalitsa Mabaibo aŵili a Ciheberi . “ Colinga cokulamulila zimenezi n’cakuti tikhale ndi cikondi cocokela mumtima woyela , m’cikumbumtima cabwino . ” — 1 TIMOTEYO 1 : 5 Makolo ambili amakonda kukambilana ndi ana awo nkhani za mu Galamukani ! Komabe , ngati mlongo wapita ndi mwamuna wosabatizidwa kukacititsa phunzilo la Baibulo lokhazikika , ndipo mwamunayo si mwamuna wake , iye safunikila kuvala cakumutu monga mmene Malemba amakambila . Kucokela nthawi imeneyo , m’malo moyambana , timasangalala kukambilana nkhani za m’Baibulo . Iye anati : ‘ Ndinaona ngati a dokotala andinamiza cifukwa ndinali wacinyamata . ’ Onjezelani nchito yanu yolalikila uthenga wabwino ndi kuphunzitsa ena Baibulo . Cifukwa cakuti salaka - laka zinthu zimene sangakwanitse , sakhala na nkhawa kwambili komanso savutika maganizo . Ngati munthu anafedwa mnzake wam’cikwati , amavutika kwambili na cisoni nthawi yoyamba pamene acita yekha zinthu zimene anazoloŵela kucita ndi mnzakeyo . Ndithudi , umoyo kumeneko unali wosiyana ngako na wa ku mudzi kwathu . Kenako , Paulo anati : “ Mwa ‘ cifunilo ’ cimeneco , tayeletsedwa kudzela m’thupi la Yesu Khristu lopelekedwa nsembe kamodzi kokha . ” ( Aheb . Poganizila zimenezi , mlongo angaone kuti n’zosatheka kukwatiwa “ mwa Ambuye . ” Kumeneko , anaona zithunzi zamalisece . Masiku ano anthu amene amagona ndi amuna kapena akazi anzao amagwilitsidwa nchito mu zosangulutsa pa nkhani ya kavalidwe n’colinga cofuna kuonetsa kuti khalidwe lao ndi lovomelezeka . Mu 1961 , m’bale wokhulupilika ameneyu anakukila ku tauni ya Kant , imene ili pafupi kwambili na kwathu . Kunena zoona , Yehova ni Tate wacikondi , ndipo amatitonthoza tikakumana ndi mavuto . Gwilitsilani Nchito Bwino Lilime Lanu Mwamuna wina amene ni kholo anavomeleza kuti : “ Nthawi zina nimapezeka kuti niganizila zinthu zina pamene ana anga akamba na ine . Koma malinga na mmene zinakhalila , mzindawo unali wosatetezeka . ( Numeri 14 : 2 - 4 , 11 ) Yehova anali kudziŵa kuti Aisiraeli sanali kum’khulupilila cifukwa io anadandaula za utsogoleli wa Mose ndi Aroni , amuna amene anasankhidwa ndi iye . Cifukwa cimodzi n’cakuti anthu a Mulungu amayesetsa kusunga lamulo la m’Baibulo lakuti : “ Cititsani ziwalo za thupi lanu padziko lapansi kukhala zakufa ku dama , zinthu zodetsa , cilakolako ca kugonana . ” ( Akol . YEHOVA ndi woyenela kumuyamikila , cifukwa amapeleka “ mphatso iliyonse yabwino ndi yangwilo . ” ( Yak . 13 : 1 , 2 ; 74 : 10 ; 89 : 46 ; 90 : 13 ; Hab . M’malomwake , zinthu zilizonse zabwino , maluso , kapena mphamvu zimene tili nazo ni mphatso zocokela kwa Mulungu , ndipo iye amakondwela ngati tizigwilitsila nchito moyenela . Ahabu anaitanitsa Naboti ndi kumuuza kuti akufuna kugula mundawo . ( Mlaliki 12 : 1 ) Koma makolo acikristu ndi akulu mumpingo amafuna kuti acinyamata amvetsetse tanthauzo la kubatizidwa ndi kuti asankhe okha kubatizidwa . Tikukhala m’dziko la Satana ndipo ndife opanda ungwilo . Kodi Yehova amauona bwanji utumiki wathu kwa iye ? Tsopano zofalitsa zimamasulidwa m’Cikigizi ndi kagulu ka omasulila amene ali pa ofesi ya nthambi ku Bishkek . “ Pamene Akhiristu anzathu anatiuza kuti anationa pa TV tikufotokoza molimba mtima za cikhulupililo cathu , tinawauza kuti zimenezo zinatheka cifukwa ca mapemphelo awo ambili - mbili amene anali kutipelekela . Iye sanali kubeleka . Upainiya unaniphunzitsa kudalila Yehova , ndipo mantha oopa kukatumikila kudziko lacilendo anatha . 6 : 6 - 9 ) Ngakhale masiku ano , malamulo a Mulungu amatiteteza ndi kutipindulitsa , ndipo ndi osavuta kutsatila . Pamene Yesu anauza atumwi kuti adzamuthaŵa kwa kanthawi , Petulo anadzikweza pamaso pa ena mwa kunena kuti iye yekha sadzathaŵa . ( Mat . Tikuitanila anthu ku msonkhano n’tangoyamba upainiya ku Ireland ( munsi ) Baibo imakamba kuti : “ Cifukwa malipilo a ucimo ndi imfa , koma mphatso imene Mulungu amapeleka ndi moyo wosatha kudzela mwa Khristu Yesu Ambuye wathu . ” — Aroma 6 : 23 . Koma ena ndi aciphamaso , amabisa zoipa zimene amacita n’kumadzionetsa monga anthu acilungamo . Kuli ofalitsa 96,000 amene akulalikila uthenga wabwino , ndipo anthu 229,726 anapezeka pa Cikumbutso mu 2013 . Ciŵelengelo cimeneci cikusonyeza kuti munthu mmodzi pa anthu 48 alionse ku Cuba anapezeka pa Cikumbutso . Kamnyamatako kanali kusankha ndalama ya siliva na kuthaŵa . Pa zifukwa zimenezi abale ena atengela anzawo kukhoti . Koma Buku la Mau ake a Mulungu limatilangiza kuti ciliko bwino kuluza cinacake kusiyana n’kubweletsa citonzo pa dzina la Mulungu , kapena kusokoneza mtendele wa mpingo . Anakamba zimenezi malinga ndi ulosi wa Danieli wonena za mtengo waukulu umene unadulidwa ndi kuphukanso patapita “ nthawi zokwanila 7 . ” N’zoona kuti tili na ufulu wosankha zimene tifuna kuvala . Koma pa Ciwelu caciŵili mwezi ulionse , tonse tinali kudyela pamodzi cakudya monga banja . Sauli ndi anthu ake anasowa mtengo wogwila cifukwa ca Goliyati . 7 : 1 , 7 ) Kodi io anali ndi colinga cotani ? Kumbukilani kuti anthu a m’midzi ya ku Simeulue , anathaŵila ku mapili mwamsanga atangoona zizindikilo pa nyanja . Colinga ca Mulungu cinasokonezeka pamene anthu anapandukila ulamulilo wake . Mau ake amakamba kuti : “ Musamade nkhawa ndi kanthu kalikonse , koma pa ciliconse , mwa pemphelo ndi pembedzelo , pamodzi ndi ciyamiko , zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu . Mukatelo , mtendele wa Mulungu umene umaposa kuganiza mozama kulikonse , udzateteza mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu . ” Ndithudi , Mau a Mulungu apitiliza kukhalapo ngakhale kuti zinenelo zakhala zikusintha - sintha . Ngati munthu wina wakamba kuti malamulo enaake afunika kucotsedwa kapena kusinthidwa , sititengako mbali , ndipo sitimulimbikitsa kusintha maganizo ake . Si Yosefe yekha amene anali na mantha . ( a ) Kodi ufulu wocita zinthu umatipatsa dalitso lapadela liti ? Malamulo a Mulungu pa nkhani ya mavalidwe amationetsa kuti iye amadana ndi masitayelo opangitsa amuna kuoneka monga akazi , akazi kuoneka monga amuna , kapena amene amasokoneza kuti ni mwamuna kapena mkazi . * N’zokondweletsa kuti lomba Baibo kapena mbali yake , yamasulilidwa m’zinenelo pafupi - fupi 3,000 . Timawakonda kwambili alongo athu amenewa . Ndi pangano liti lopezeka m’Baibulo limene limapangitsa kuti zikhale zotheka kuti anthu ena akalamulile ndi Kristu ? Anthu amene amaphunzila za ubwenzi wa pakati pa anthu apeza kuti “ anthu amene nthawi zonse amaganizila anzawo , amalimbikitsa ena kutengela khalidwe lawo . ” Masiku ano , iye ndi womasuka kwambili . ” Tonse tinali okwiya ndipo zinali zovuta kukambilana nkhaniyi mwamtendele . Conco , ndinacita kuwalembela makalata powafotokozela zolinga zanga . Pakapita nthawi anali kufalitsa khadi lina lokhala ndi uthenga watsopano . Iwo saopa kuti ena angaleke kuwapatsa ulemu cifukwa cosintha zimene anasankha . Akulu afunika kukhala okonzeka kusintha maganizo awo ndi zosankha zawo ngati m’pofunika . M’bale Mumba : Tiyeni tiyambe ndi Yohane 14 : 6 kuti timve zimene Yesu iye mwini ananena . 16 , 17 . ( a ) Kodi ufulu wosankha unakhala bwanji vuto kwa Akhiristu a ku Korinto ? 6 : 20 ) Kunena zoona , ubwenzi wathu ndi Yehova ndiye cinthu camtengo wapatali kuposa zonse zimene tingakhale nazo . M’kupita kwa nthawi , ife Mboni tinagaŵana m’tumagulu kuti tsiku lililonse tizikambilana lemba limene wina waganizila . Kodi kukhala munthu wauzimu kungatithandize bwanji ( a ) kupewa zolinga zosapindulitsa ? Nanga n’cifukwa ciani zimenezi siziyenela kutidabwitsa ? ( b ) N’ciani cidzacitikila Satana ? Movutikila , iye akupeza malo okhala mu holo imene mukukambidwila nkhaniyo . Muyenela kukhutila kuti mwapeza coonadi . Koma maganizo awo anali wolakwika . ( Yesaya 48 : 17 ) Iye amatiuza zimenezi kudzela m’Mau ake , Baibulo . Titatsala pang’ono kufika m’malile a dziko la Greece ndi Albania , mwadzidzidzi asilikali a Greece anatizungulila . N’zosakayikitsa kuti mbalame zimene zinali kumanga zisa zawo pa kacisi caka ciliconse , zinali kukhala zotetezeka ndipo zinali kulela ana awo popanda cosokoneza . “ Nowa , Danieli ndi Yobu , . . . iwo okhawo akanapulumutsa miyoyo yawo cifukwa cokhala olungama . ” — EZEK . Zimenezi zimam’thandiza kudziŵa mfundo zina zimene sizidziŵika mwamsanga . Komanso pokamba ndi wopelekela cikho , anafotokoza mosapita m’mbali zimene zinamucitikila podziŵa kuti mnzakeyo akanamuthandiza . Ndipo zingakhale zovuta kwambili kukamba na gulu la anzanu kusukulu kusiyana na kukambilana na mnzanu mmodzi wa m’kilasi . Mfundo Zimene Atsogoleli Acipembedzo Aciyuda Anali Kutsatila Pofuna Kuthetsa Cikwati , Na . Pambuyo pake , anatiuza kuti , “ Cabwino , nidziŵa kuti simungakane kusamalila nkhosa . M’malo mothetsa cilakolako coipaco , iye anacilekelela mpaka cinakula ndi kubala chimo . ( Yak . Oyang’anila dela amayamikila kwambili ngati abale ndi alongo amawakonda kucokela pansi pa mtima , ndi kukhala mabwenzi ao enieni . Mwa zokamba zao ndi kavalidwe kao , acinyamatawa amasonyeza kuti salemekeza acikulile ndipo amawaona kuti ndi “ otsalila . ” M’kupita kwa nthawi , tinatumizidwa kuti tikatumikile m’dela lina la kufupi na dziko la Brazil . Nthawi yoyamba pamene ndinakumana ndi Kingsley , ndinacita cidwi kuona kuti anali ndi njala ya coonadi . Msilikali ameneyu , amene anali kuonedwa monga mdani , anali kulalikila za mtendele kwa anthu okamba Cifulenchi atavala yunifomu yausilikali . MUNTHU akagwila bwino nchito imene wapatsidwa , kapena akacita zinthu zoonetsa khalidwe linalake losililika , amafunika kutamandidwa . ( Aroma 15 : 7 ) Koma ku misonkhano kukabwela acatsopano , na ise timakhala m’gulu la olandila alendo . Komabe , kumbukilani kuti ngati tikamba , “ tonsefe timapunthwa nthawi zambili . ” ( Yak . Yesetsani kuona zimene mungaphunzilepo inu panokha ndi banja lanu . Mwana angagwilitsile nchito liu limeneli poitana atate wake mwacikondi ndi mwaulemu . Mtumwi Paulo anawalembela kuti : “ Musamangidwe m’goli ndi osakhulupilila , cifukwa ndinu osiyana . ” Mwinanso zinali zovuta kwa Sara kuti asiye nyumba yake . Munthuyo anakhudzidwa ngako na lembali cakuti anapempha m’baleyo kuti aŵelengenso lembalo . Sembe iwo anakhala na maganizo amenewo , akanabwelela ku Uri , ndipo akanataya mwayi waukulu umene Yehova anali kudzawapatsa . Anagwila mtembo wa mwanayo na kupemphela kwa Mulungu kuti : “ Mulungu wanga , conde cititsani kuti moyo wa mwanayu ubwelele mwa iye . ” Onelelani vidiyo yakuti , N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo ? Yesu anali kukamba za nthawi yaitali imeneyi pamene anati Akristu onama , amene ndi namsongole , adzakulila limodzi ndi “ ana a Ufumu ” amene ndi tiligu . Mwa tsoka lanji , amayi anapezeka na matenda a khansa . Kodi naonso adzasangalala panthawiyo ? ( Ŵelengani 1 Akorinto 14 : 33 , 40 . ) ( Mateyu 22 : 37 - 39 ) Tikamalalikila uthenga wa ufumu timaonetsa kuti tikumvela malamulo amenewa . — Ŵelengani Machitidwe 10 : 42 . Ngati tate amakonda ana ake , naonso amayamba kum’konda . 1 , 2 . ( a ) Kodi amene amatsogolela pakati pa Mboni za Yehova amasiyana bwanji ndi atsogoleli a m’machechi ena ? Ndinali kufunitsitsa kuyeletsa dzina la Yehova ndipo ndinali kufuna kuti mwana wanga adzaonanenso ndi atate wake m’paladaiso . ” — Miy . Lamulo limakhudza cabe mbali imodzi , koma mfundo imakhudza mbali zambili mu umoyo . Baibulo limayankha kuti : “ Abale ake ataona kuti bambo ao anali kukonda kwambili Yosefe kuposa io onse , anayamba kudana naye cakuti sanali kulankhula naye mwamtendele . ” Tingaonetse bwanji kuti tili ndi cikhulupililo colimba ? ( Miy . 1 : 5 ) Ndani angakuthandizeni kudziŵa nchito imene mungasankhe pogwilitsila nchito mfundo za m’Baibo ? Ngalazo zinali zonyala ndi zowauka , ndipo zinameza ngala 7 zazikulu bwino zija . Kutaca m’mawa , Farao anavutika kwambili maganizo . Ganizilani zimene Akhristu amene ali pabanja angacite kuti atengele citsanzo ca Yehova ndi kucilikiza ulamulilo wake . TAYELEKEZANI kuti mukuona Yesu atakhala pa Phiri la Maolivi , ndipo akuyang’ana kacisi amene ali mu Yerusalemu . M’nthawi zakale , Yehova anali kuteteza anthu ake akamathandizana panthawi za mavuto . 1 , 2 . ( a ) Kodi atumiki a Mulungu ali na ciyembekezo canji ? Vesi 20 ionetsa kuti Yehova anawapatsa mpata woonetsa zimene zinali m’mitima yawo . Ndiyeno , cinthu cina cosangalatsa cinacitika . ( b ) Kodi Samueli anaigwila bwanji nchito yodzoza Sauli ? Mwamuna wake atamulola , iye anayenda ulendo wa makilomita pafupifupi 30 kupita ku Phili la Karimeli , kumene kunali Elisa . Ife alambili a Yehova tiyenela kutsatila citsanzo ca Nowa ndi banja lake , ndiponso Akristu oyambilila amene anali omvela . 13 N’cifukwa Ciani Tiyenela ‘ Kukhalabe Maso ’ ? Conco , Mulungu anam’gonetsa tulo tofa nato , n’kumucotsa nthiti imodzi imene anapangila mkazi , na kum’bweletsa kwa iye . Cifukwa cakuti munthu amafunika kupilila kuti apitilize kukhala wotsatila woona wa Khristu . Nanga kukhala Mkristu kungabweletse mavuto otani ? 9 Kodi Cidzacokapo N’ciani Ufumu wa Mulungu Ukadzabwela ? Zakhaladi zosangalatsa kuphunzila za makhalidwe a Yesu ocititsa cidwi . Tingaphindule kwambili kuphunzila za makhalidwe ake ena ndiponso kuyesa kutengela citsanzo cake . ( a ) Kodi mzimu wa Yehova ungatimasule ku ciani ? Mwa ‘ kulolelana m’cikondi ndi kuyesetsa na mtima wonse kusunga umodzi wathu mwa mzimuwo , ndi mwamtendele , ’ tingakhululukile na mtima wonse anthu amene anatilakwila mosadziŵa . ( Aef . Onelelani vidiyo yamutu wakuti , Special Convention in Israel pa webusaiti yathu ya www.jw.org , ndipo onani mmene Mboni za m’dziko la Israeli ndi Palestine zapewela kusankhana mitundu . Anali wokonzeka kucita zimenezo ngakhale kuti anali atauzidwa kuti : ‘ Amene adzachedwa “ mbeu yako ” adzacokela mwa Isaki . ’ Pomaliza M’bale Julian anati : “ Kucotsa munthu mumpingo ndi makonzedwe abwino amene amatithandiza kutsatila miyezo ya Yehova pa umoyo wathu . Mwina tingaŵelenge naye lemba la Yohane 6 : 38 , pamene Yesu anati : “ Ndinatsika kucokela kumwamba kudzacita cifunilo ca iye amene anandituma , osati cifunilo canga . ” Tsopano , ndimasankha zakudya zogula , ndipo ndimafunafuna zochipa . Komabe , pali zambili zimene mungacite kuti muwateteze . Iye anali kutanthauza kuti malinga ngati dziko loipali lilipo , anthu osauka adzakhalapobe . Mulungu ali ndi thupi lauzimu ndipo sitingamuone . Tiyenela kudzifunsa kuti : ‘ Munthu uyu wakamba kuti cakudyaci kapena mankhalawa anathandiza anthu ena ake , koma kodi pali umboni wosonyeza kuti anawathandizadi ? Koma ndine ndani kuti nicite zimenezo ? ” — Yesaya 40 : 8 . Inde , timafuna kuti ana athu komanso ophunzila Baibo apite patsogolo mpaka akabatizike . N’cifukwa ciani tiyenela kuganizila zinthu zabwino zimene tili nazo tikakumana ndi mavuto ? Ndipo anacita ciani kuti alithetse ? Amai anapempha anthu ena kuti andinyengelele kusintha maganizo anga . Cathy anati : “ Nthawi zonse ndimapemphela kwa Yehova kuti ndikhale wokhutila ndi zimene ndimadya ndi zovala zochipa zimene ndimavala . Ngati anthu afikila akulu kuti awathandize pa mavuto a m’banja , akuluwo angacite bwino kuwafunsa ngati posacedwapa anaonelelako monga banja vidiyo yakuti Chikondi Chenicheni . Kakambidwe kanga sikanali kabwino , ndipo n’nali kukonda nthabwala zotukwana . Mwina takhala tikulimbana ndi cofooka cimeneco kwa zaka zambili . Ngati munatula udindo wanu wotumikila nkhosa za Mulungu , zingakhale bwino kudzifunsa cifukwa cimene munacitila zimenezo . Taganizilani zitsanzo zitatu izi . ( Dan . 8 : 5 - 7 , 20 , 21 ) Pamene ufumu wa Girisi unakula , anthu ambili a mu ufumuwo , kuphatikizapo Ayuda amene anali m’madela osiyana - siyana , anayamba kukamba Cigiriki . Ngakhale kuti likulu lathu lili ku United States , Mboni za Yehova zambili zimakhala m’maiko ena . Koma dziŵa izi : Kaya munthu amavomeleza za Mulungu kapena za cisanduliko , nkhani ya cikhulupililo imakhalapo ndithu . Nowa anali munthu wabwino , koma sanangokhutila na zimenezo . Tiphunzilapo ciani pa zimene Yehova anauza Mose ponena za tanthauzo la dzina lake ? ( Salimo 13 : 1 ) Koma pamene Davide anazindikila kuti Yehova anam’teteza nthawi zambili , cidalilo cake mwa Mulungu cinakula . Zoonadi , tidzayamikila kwambili kuti Mulungu amene ‘ anaika nthawi kapena nyengo pansi pa ulamulilo wake , anatilangiza kukhala maso popeza ‘ mapeto a zinthu zonse anali atayandikila . ’ — Mac . 1 : 7 ; 1 Pet . ( Yobu 34 : 21 , 22 ) Kukamba zoona , palibe amene angathawe ciŵeluzo ca Yehova Mulungu . Ndi Satana ! Iye alibe ciyembekezo ndipo amafuna kuti nafenso tizidziona kuti tilibe ciyembekezo . Kuti tilandile madalitso a Mulungu , tifunika kutsatila malangizo amene iye amatipatsa kudzela mumpingo wacikristu . Kuti alambile Yehova ndi kum’tumikila movomelezeka , kodi anthu amene si Aisiraeli a kuuzimu afunika kucita ciani ? Nanga zimenezi zinanenedwelatu motani m’Baibulo ? Anali kutikonda monga tate ŵathu ndipo zimenezi zinatilimbikitsa mwauzimu . Ndine wofunitsitsa kukuthandiza . ” Kuyambila mu 1914 , mbali ya padziko lapansi ya gulu la Mulungu yakhala ikukula modabwitsa . 6 , 7 . ( a ) Kodi mphepo yamkuntho ndi mafunde zimene zinacititsa mantha Petulo tingaziyelekezele ndi ciani ? Asilikali a Japan atatsala pang’ono kuukila dziko la India , akulu - akulu a dziko la Britain amene anali kulamulila dzikolo , anayamba kuvutitsa kwambili Mboni za Yehova . Anacenjeza kuti ngati munthu akonda kwambili zinthu za m’dzikoli “ monga cilakolako ca thupi , cilakolako ca maso ndi kudzionetsela ndi zimene munthu ali nazo pa moyo wake ” ndiye kuti “ sakonda Atate . ” M’dziko latsopano la Mulungu tidzakhalanso ndi nthawi yosangalala ndi zinthu zimene timakonda . Ganizilani coyamba liu lakuti “ thupi . ” N’tangomuona , n’nam’konda kwambili , cakuti tinakwatilana tsiku lomwelo . Anali kuikonda kwambili nchitoyo . Adzadziŵa kuti mumamulemekeza ndipo mumadziŵa kuti iye akufika pa ucikulile . Yesu anali ndi moyo monga colengedwa cauzimu camphamvu cimene munthu sangaphe . Kodi acicepele ena acikhristu acita zotani kuti acite zambili pa nchito yopanga ophunzila ? Koma anagona ndipo anagwa kucoka pa nyumba yacitatu yosanja mpaka pansi . Ndinasokonezeka maganizo kwambili . Komanso zimaphatikizapo zinthu zina zimene mumacita monga kupemphela panokha kwa Yehova ndi kucita phunzilo laumwini . Iye anayesa kukopa anthu opitilila 1,000 amene anali kumvetsela kuti ayambe kutsutsa Ophunzila Baibo . Baibulo limati : “ Valani cifundo cacikulu , kukoma mtima , kudzicepetsa , kufatsa , ndi kuleza mtima . Ndipo odzimvela cisoni mumtima mwawo amawapulumutsa . ” ( Sal . Baibo siiletsa kumwa moŵa mwacikati - kati , koma imati : “ Usakhale pakati pa anthu omwa vinyo kwambili . ” M’bale wina wa m’komiti yoyang’anila za cithandizo anati : “ Abale ocokela m’madela osiyanasiyana m’dziko la Japan anacita zinthu mogwilizana pothandiza abale athu . Anamasuka Kucoka ku Cipembedzo Conama , Nov . Komanso , ena amakhulupilila kuti mahomoni a m’ma IUD amenewa amapepukitsako cibalilo . Dzina limeneli ndi loyenelela cifukwa colinga ca nyuzipepala imeneyi ndico kuuzako ena zenizeni zimene zimacitika . Kuwonjezela apo , monga tate wacifundo , Mulungu afuna kuti ise ana ake , tiziona zolakwa mmene iye amazionela . Ndinacoka panyumba ndi kukakhala mumzinda wa Zanesville ku Ohio , koma ndinali kupitabe kunyumba kaŵilikaŵili kukalimbikitsa acibale anga . Ngati mumalemekeza ena na kuwaonetsa cidwi , iwonso adzacita cimodzi - modzi kwa inu . Mwina adzayesa kucititsa anthu kukhulupilila kuti akhoza kukhala na moyo wosatha popanda kumvela Yehova . Mikhail anapitiliza kuti : “ M’dela limenelo tinapezanso kagulu ka azimai ena pafupifupi 10 a chechi ca Baptist amene anali ndi njala ya coonadi . Koma panthawi yovuta imeneyo analola kuti Yehova amutsogolele . Koma kutalikitsa moyo mwa njila imeneyi sikutanthauza kuti munthuyo wacililatu . Ngati n’conco , dziŵani kuti Yehova amakudelani nkhawa . Tonse kaya ndife odzozedwa kapena a nkhosa zina , tiyembekezela kuona kukwanilitsika kwa colinga cimene Mulungu anali naco poyamba , ndi kuyeletsedwa kwa dzina lake . ( Yoh . 10 : 16 ; Mat . Herd Iye anaona kuti mwamunayo alinso ndi ngamila 10 zimene zinali gone pafupi ndi comwelamo ziŵeto , cimene munalibe madzi . 11 ELIAS HUTTER NA MABAIBO AKE A CIHEBERI OCITITSA CIDWI Cifukwa ca khama lake ndi thandizo la mzimu woyela wa Mulungu , Petulo anagonjetsa mtima wodzikonda ndipo anaonetsa kudziletsa ndi cikondi codzimana . Pa cikwati ca Mwanawankhosa , “ iye waloledwa kuvala zovala zapamwamba , zonyezimila ndi zoyela bwino , pakuti zovala zapamwambazo zikuimila nchito zolungama za oyela . ” — Chiv . Ambili amapeleka mayankho osiyana - siyana pa funso limeneli . Koma kodi n’kuti kumene tingapeze yankho lodalilika ndi loona pa funso logometsa mutu limeneli ? Paliponse tingoona a Mboni za Yehova . ’ ” Nkhani zimenezi zifotokoza bwino mbali ziŵili za cikhulupililo zofotokozedwa pa Aheberi 11 : 1 . Kuti munthu akhale paubwenzi ndi Mulungu sayenela cabe kudziŵa kuti Yesu ndi Mpulumutsi . Kodi mungayeseko kucita zimenezi ? M’bale John anati : “ N’nali wotangwanika na nchito yabwino kwambili kuposa ina iliyonse imene n’nagwilako . Analinso ndi nyumba ina ku Yezereeli , dela limene linali pa mtunda wa makilomita pafupi - fupi 37 kucokela ku Samariya . Atafika zaka 40 , iye anaona kuti angakwanitse kumasula anthu a Mulungu ku ukapolo mu Iguputo . ( Mac . Ndinaphunzitsidwa kuti mkazi afunika kugwila nchito ku khichini , kusamalila mwamuna , ndi ana . Ngakhale kuti a nkhosa zina alibe ciyembekezo ca kumwamba , naonso angaike maganizo ao pa zinthu zakumwamba . Ali kumeneko , anakwatila amayi , ndiyeno mu 1953 ine n’nabadwa . ( 2 Mbiri 18 : 1 - 32 ) Zitatelo , mneneli Yehu anafunsa Yehosafati kuti : “ Kodi cithandizo ciyenela kupelekedwa kwa oipa , ndipo kodi muyenela kukonda anthu odana ndi Yehova ? ” — Ŵelengani 2 Mbiri 19 : 1 - 3 . 11 : 35 ) Ngakhale kuti sindife otsimikiza za anthu amene Paulo anali kukamba , ena monga Naboti na Zekariya , anaphedwa mwa kuponyedwa miyala cifukwa comvela Mulungu ndi kucita cifunilo cake . ( 1 Maf . Lemba la Salimo 40 : 8 linaonetselatu kuti Yesu adzakhala munthu wokonda cilamulo ca Mulungu . Pa lembali pamati : “ Ndimakondwela ndi kucita cifunilo canu , inu Mulungu wanga , ndipo cilamulo canu cili mumtima mwanga . ” Ngakhale kuti tinalonjezedwa zakudya zambili ndi zinthu zina zabwino m’dziko latsopano , tidzasangalalanso kwambili pamene zosowa zathu zakuuzimu zidzakhutilitsidwa . ( Mat . Koma koposa zonse , Yesu anali kum’konda cifukwa cakuti anali ndi cikhulupililo colimba . Kodi Mulungu Amakuona Bwanji Kukoka Fodya ? Naoko , amene tam’chula m’nkhani yapita , anafotokoza cimene cinam’thandiza kuti aleke kukoka fodya . Chivumbulutso 6 : 7 , 8 Fajardo ) , Dec . ( Aroma 12 : 2 ) Ndinali munthu waciwawa , wamkali ndipo ndinali kukhalila kunama mabodza . Akristu ena odzipeleka kwa Mulungu analoŵelela m’ndale . Nkhalango ya Biriya ya ku Galileya ( pansipa ) 1 : 8 ) Mwacionekele , otsatila a Kristu oyambilila anadziŵa zimene anafunikila kucita . Iye anawauza kuti : “ Mulungu amakonda munthu wopeleka mokondwela . ” — 2 Akorinto 9 : 7 . KUYAMBILA kale , anthu a Mulungu akhala akupeleka nsembe monga mbali ya kulambila koona . Ndipo iye anagwilitsila nchito mpata umenewu kuwaphunzitsa kuti ngati aika maganizo ao pa kukhala ndi zinthu zambili , zingawasokoneze kutumikila Mulungu . — Luka 12 : 13 - 15 . Ulaliki unayenda bwino ndipo n’napeza cimwemwe coculuka . Nanga bwanji ngati munthu wakhala mlambili wa Yehova ali kale pa banja ndi munthu wosakhulupilila ? Baibulo limati : “ Amene anaphedwa anali oculuka kwambili . Panaphedwa amuna oyenda pansi a Isiraeli okwanila 30,000 . N’cifukwa ciani tiona kuti n’zotheka kuonetsa cikondi kwa anzathu ? 2 : 26 , 27 ) Motelo , magulu a nkhondo a kumwamba a Kristu adzaphatikizapo abale ake odzozedwa amene panthawiyo adzakhala kuti alandila mphoto yao kumwamba . 6 , 7 . ( a ) Ndi makhalidwe ena ati amene amaonetsa kuti Mkristu ndi wofikapo ? Kodi mlongo wina wacitsikana anakamba ciani za mphatso yocokela kwa Yehova ? Tingathandize bwanji anthu amene ali monga bango lophwanyika kapena cingwe ca nyale comwe catsala pang’ono kuzima ? Koma malinga ndi zimene Bungwe Loona za Umoyo pa Dziko Lonse linakamba , anthu ambili amafa ndi matenda opatsilana monga TB cifukwa cokoka . Munthu aliyense afunika kucenjezedwa mapeto asanafike . — Mateyu 24 : 14 . ( Agalatiya 5 : 22 ) Ngati titsatila malangizo a Yesu akuti tizipempha kuti ationjezele mzimu woyela , ndiye kuti ticita zinthu mwanzelu . Iye “ anatsegulilatu maganizo ao kuti amvetse tanthauzo la malemba . ” Kuti mudziŵe zambili pa nkhani yophunzitsa ana ngati mnzanu wa m’cikwati si Mboni , onani “ Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga ” mu Nsanja ya Olonda , ya August 15 , 2002 . Pofotokoza makonzedwe amenewa , Utumiki Wathu wa Ufumu wa October 2008 unati : “ Mitu ya mabanja iyenela kukwanilitsa udindo umene Yehova anawapatsa poonetsetsa kuti akuphunzila Baibulo ndi banja lao nthawi zonse . ” Anthony Hambuch analemba kuti : “ Alimi anakonza bwalo m’munda wa zipatso ndi kupanga mabenchi a mitengo kuti anthu azisangalala ndi filimuyo . ” 27 : 23 . Kodi munakhumudwa cifukwa ca zophophonya za ena ? ( Aroma 12 : 9 ) Tingadzifunse kuti : ‘ Kodi kucita zosangalatsa zimenezi kudzaonetsa kuti ndine wacinyengo ? Conco , musamamvetsele mauthenga osoceletsa a Satana . Ndinali kugwila nchito za panyumba , ndipo madzulo alionse tinali kupemphela pamodzi pemphelo la Korona . Nthawi zina , akulu aŵili angafikile mlongo wofunika thandizo na cilimbikitso ca m’Malemba . Mungacite bwino tsiku lililonse kudzifunsa kuti , ‘ N’ciani cimene ningawongolele lelo kuti nipite patsogolo mwauzimu ? ’ Komabe , iye anali kufunitsitsa kudziŵa tanthauzo la malotowo . Onani nkhani yakuti “ Mungathe Kuphunzira Chinenero China ! ” ( Aroma 7 : 25 ) N’zoona kuti Paulo anali kulimbana na ucimo , ndipo analakwitsapo zinthu zina . ( Mat . 6 : 19 , 20 ) Riana anakukila ku dela la kum’mwela kweni - kweni kwa dzikolo , kumene kumacitika cilala kaŵili - kaŵili . Koma iwo anatikakamiza kuyenda na mendo kupita ku Phili la Olympus , limene lili pamtunda woyenda maola 12 kucokela m’mudzi wathu . Kodi ndinu wosakwatila kapena wosakwatiwa , ndipo mumafunitsitsa kugwilitsilidwa nchito m’gulu la Yehova ? Kutaikilidwa Atate , Kupeza Atate ( G . Mwina Petulo anaganiza kuti iye ndiye adzakhala pa malo apamwamba amenewo popeza Yesu anali atanenapo kuti Petulo adzapatsidwa udindo wapadela . Ambili a inu abale na alongo okondedwa mukuvutika na matenda aakulu . ( Miy . 17 : 27 ) Phunzilani kucita zinthu mwaucikulile . Muzilandila uphungu moleza mtima , na kuuseŵenzetsa popanda kudandaula na mmene wapelekedwela . ( Miy . Conco , tikakhala na nkhawa , tifunika kumuuza Yehova nkhawa zathuzo m’pemphelo . Iye anali kufunitsitsa kuti munthu aliyense akhale na mwayi wopindula na Mau a Mulungu . Muzisinkhasinkha za Cikondi Cosatha ca Yehova Mwacitsanzo , Baibulo la Cingelezi linagwilitsila nchito mau Aciheberi akuti “ Shelo ” pa Mlaliki 9 : 10 komanso m’mavesi ena . Pa tsikulo anthu anatseka mabizinesi ao ndipo anali kuvina m’miseu . Tiyenela kufuna - funa mipata yoyamikila ena cifukwa kucita zimenezi ‘ kumalimbikitsa . ’ ( Aef . NYIMBO : 123 , 128 Panali atumiki okwana miliyoni imodzi amene anali kumutumikila nthawi zonse , ndi atumiki enanso mamiliyoni 100 amene anali kuimilila pamaso pake nthawi zonse . ” — Danieli 7 : 9 , 10 . Yehova adzasamalila zimenezo . 16 : 21 ) Kodi mwina ndiye cifukwa cake anaganiza kuti Ayudawa , Paulo na Sila , sangakhale nzika za Roma ? ( Mat . 24 : 13 ) Zoonadi , ngati tikhalabe okhulupilika tidzapulumuka . Iwo sanafune kuphunzila , koma pofuna kuonetsa ulemu anawauza kuti aziphunzila ndi ine . mu Galamukani ! ya February 2013 . Cifukwa cakuti Mose anali ndi cikhulupililo . Mlongo wina wocokela ku Australia , dzina lake Trazel , amene ali na zaka za m’ma 50 , wakhala akutumikila ku Myanmar kuyambila mu 2004 . Ezekieli analemba mau a m’lemba la mutu wa nkhani ino mu 612 B.C.E . * ku Babulo . M’macaputala amenewa , Baibulo limatiuza za “ ciyambi , ” pamene zinthu monga milalang’amba , nyenyezi , ndi dziko lapansi zinalengedwa zaka mabiliyoni ambili zapitazo . N’cifukwa ciani Mulungu anasankha Mariya kuti adzakhale mayi wa Yesu ? M’Baibo , mitu ya mabanja imalangizidwa kuti : “ Musamapsetse mtima ana anu , koma muwalele m’malangizo a Yehova ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe kake . ” ( Aef . Posacedwa , Mulungu adzawononga Satana ndi kukwanilitsa cifunilo cake padziko lapansi . Ena amasoŵa cocita ndipo amafooka . Zimenezi zingapangitse vutolo kukulila - kulila . Mwacitsanzo , ganizilani mfundo iyi ya m’Baibo yakuti : “ Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila . ” Kusinkhasinkha za Yehova ndi Yesu kudzakuthandizani kukhalabe wacangu potumikila Mulungu . Kenako iye anapeza njila yocitila zimenezo . Baibo imayankha kuti : “ Nyumba iliyonse inamangidwa ndi winawake , koma amene anapanga zinthu zonse ndi Mulungu . ” — Aheb . Ise atumiki a Mulungu tifunika kusamala kuti tisayambe kutengela makhalidwe oipa a anthu ena . Kuŵelenga ndi kuonelela zinthu zoipa kudzatha posacedwapa . Mwacitsanzo , ngati wina wadzipeleka kuti atilipilile cithandizo ca ku cipatala kuti apulumutse moyo wathu , cimene ife sitingakwanitse kulipila , timayamikila kwambili . M’dziko latsopano , anthu onse adzakhala pansi pa ulamulilo wa Yehova , ndipo adzaphunzila njila zake zolungama . ( Yes . 10 : 35 , 36 ) Conco , tiyeni tipitilize kulimbitsa cikhulupililo cathu na kutumikila Yehova ndi moyo wathu wonse . Zikusonyeza kuti mfundo za m’Baibulo zimene akulu amagwilitsila nchito pophunzitsa abale zimagwila nchito kwa wophunzila aliyense “ kulikonse mumpingo uliwonse , ” monga mmene zinalili m’nthawi ya mtumwi Paulo . ( 1 Akor . Pamene anali padziko lapansi , Yesu anaonetsa kuti iye ndi “ mphamvu ya Mulungu ” mwa kulamulila mphamvu za cilengedwe . Monique anati : “ Tsiku lina abwana anga ananiitana . Tingacitenji kuti Mulungu azititsogolela ? Koma cikhulupililo cathu cingayesedwe pamene tili tokha , monga mmene zinalili kwa Yesu m’cipululu . Komabe , ngakhale kuti tatumikila Mulungu kwa zaka zambili kapena kwa nthawi yocepa , tiyenela kupitiliza kudya cakudya cotafuna ca kuuzimu . Zamoyo zinalengedwa m’njila yabwino ndi yocititsa cidwi , ndipo zimenezi zionetsa kuti Mlengi wake ndi wanzelu kwambili . Iye anakumbukila zithunzi za nkhani za m’Baibo zokoloŵeka ku cipupa m’nyumba mwake . Aisiraeli anali kutsatila dongosolo limeneli ku Iguputo asanakhale akapolo . ( Gen . PAMENE Corinna anali ndi zaka 17 , amai ake anamangidwa , kenako anawatenga ndi kupita nao kutali . “ Kristu anaukitsidwa kwa akufa , n’kukhala cipatso coyambilila ca amene akugona mu imfa . ” — 1 Akorinto 15 : 20 . A Yohane : Kunena zoona , ndimaona kuti Baibulo ndi buku labwino , koma ndimaona kuti ndi lacikale . ( Maliko 12 : 31 ) Amuna amalamulidwa kuti ‘ azikonda akazi awo monga matupi awo . ’ Ngati timadziona mwanjila imeneyi , zingakhale zovuta kupewa zandale . Ndimacita zinthu mozindikila kuposa anthu acikulile , cifukwa ndimasunga malamulo anu . ” Munali mitengo ya zipatso imene Adamu anauzidwa kuti azidya . Ndipo amuna ndi akazi amakhala okhutila podziŵa kuti akukondweletsa Mulungu . — Aef . Koma ndife okondwa kwambili cifukwa cakuti Mulungu anatilemekeza mwa kutilola kudzisankhila tokha zocita . N’ciani cinathandiza Ribeiro kuleka cizoloŵezi cake cotamba zamalisece ? 13 : 17 ) Kucita zimenezi kudzatipindulitsa ngako cifukwa Mulungu amatifunila zabwino . Cifukwa cacinai cimene timakhulupilila kuti Yesu anaukitsidwa n’cakuti tili ndi umboni wakuti iye akulamulila monga Mfumu , ndipo akutumikila monga Mutu wa mpingo wacikristu . NYIMBO : 111 , 109 Masiku ano , pali zinthu zambili zimene zakhala zikucitika zimene zionetsa kuti Mulungu ni wacifundo . Mwacitsanzo , nthawi ina mngelo wa Yehova anapha asilikali 185,000 a Asuri . Munthu mmodzi sangakwanitse kucita zotelo , ndipo si copepuka kuti gulu la asilikali licite zimenezi . ( 2 Maf . M’malomwake , anafuna kuika Isi - boseti , mwana wa Sauli kukhala mfumu . Onelelani vidiyo yakuti Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji ? N’cifukwa ciani cikhulupililo colimba n’cofunika kuti Mkristu asacite zimene acibale akufuna ? Mofanana ndi Solomo , timafunika thandizo la Yehova kuti tikhale olimba mtima ndi kugwila nchito imene watipatsa . Kale atumiki a Yehova okalamba naonso anakumana ndi mavuto ofanana ndi amenewa . Ndiyeno , ndinatumila foni Gwen ndi kum’funsila cikwati . Nchito yathu imacilikizidwa ndi ndalama zimene anthu amapeleka mwakufuna kwao . Pangani Malemba kukhala maziko a nkhani yanu Komabe , pa nkhani imeneyi ya kukhala munthu wauzimu , palinso zina zimene tiyenela kukambilana . Ndi lemba liti limene limacititsa cidwi akatswili a Baibulo ? Nanga n’cifukwa ciani ? ( Salimo 133 : 1 - 3 ) Koposa zonse , tidzakhala paubwenzi wolimba ndi Yehova , “ Mulungu amene amapatsa mtendele . ” ( 1 Tim . 2 : 9 , 10 ) Mwinanso tingafune kumalimbikitsa njila zina zake , cabe cifukwa ca udindo wathu , maganizo athu , kapena pofuna kulimbikitsa maganizo a anthu amene timamvana nawo . Mukamuthandiza , iye angakulitse luso lake monga mphunzitsi wa Mawu a Mulungu . — Neh . Anthu a Yehova akhala akuseŵenzetsa zipangizo zamakono kuti alalikile uthenga wabwino . ( Aef . 5 : 17 ) Muziseŵenzetsa mokwanila zida zofufuzila zimene gulu la Mulungu lapeleka , monga Watch Tower Publications Index , Buku Lofufuzila Nkhani la Mboni za Yehova , Watchtower Library , LAIBULALE YA PA INTANETI ya Watchtower , na JW Laibulale . Paulo anafotokoza kuti : “ Ndikufuna mudziŵe kuti mutu wa mwamuna aliyense ndi Kristu . Mwacitsanzo , ngati takhumudwa na zokamba kapena zocita za Mkhristu mnzathu , tingacite bwino kukumbukila nthawi pamene ise tinakamba kapena kucita zinthu zimene zinakhumudwitsa ena . Coyamba , tingathandize abale athu mwa kuwapatsako cakudya , zovala , ndi zinthu zina zofunika . Zioneka kuti ena pamisonkhano yathu amakhwimitsa malamulo pankhani ya kavalidwe , pamene ena amavala motailila kwambili . Mwacikondi Yehova anateteza anthu ake m’caka ca 1513 B.C.E . Iye anapulumutsa Aisiraeli ku ukapolo ndipo anawateteza pamene anali kuwoloka pa nyanja yofiila . N’cifukwa ciani mumaona kuti kudzipeleka kumene munacita kwa Yehova n’cinthu cofunika kwambili ? Cifukwa cakuti anali kukaikilabe , Gidiyoni anapempha Mulungu kuti amupatse cizindikilo . Koma anali kucita izi cifukwa cokonda anthu mocokela pansi pa mtima . M’caka ca 49 C.E . , atumwi ndi akulu ku Yerusalemu anasonkhana kuti akambilane ngati anthu amitundu ina , amene anakhala Akhristu , anafunika kudulidwa . Amayi anakana , koma anawauza kuti mwina ine ningakonde kuphunzila . Cocitika cimeneci cidzakwanilitsa mau a pa Danieli 2 : 44 amene amasonyeza kuti Ufumu wa Mulungu “ udzaphwanya ndi kuthetsa maufumu ena onsewo . ” Kodi tidzaonetsa kuti timagwilizana ndi cilungamo Yehova ? M’dzikoli munali cabe munthu mmodzi amene anali kulandilako magazini a The Watch Tower . 3 : 14 - 16 ) Koma n’zokondweletsa n’zakuti Baibo imatipatsa malangizo a mmene tingapewele mavuto amenewa ndi kulimbikitsa mtendele mumpingo . 6 : 11 ) Kodi zimenezi zinasonyeza kuti Yehova walephela kulamulila zocitika za padziko lapansi ? Pali pano , ku Taiwan kuli abale ndi alongo oposa 100 amene akutumikila m’madela mmene mufunikila ofalitsa Ufumu ambili . Cifukwa ? Baibo imati : “ Popanda cikhulupililo n’zosatheka kukondweletsa Mulungu . Pakuti aliyense wofika kwa Mulungu ayenela kukhulupilila kuti iye alikodi , ndi kuti amapeleka mphoto kwa anthu omufuna - funa ndi mtima wonse . ” ( Aheb . 11 : 6 . ) Komanso , “ Cikondi sicitha . ” ( Aroma 5 : 12 ) Conco tinganene kuti “ malipilo a ucimo ndi imfa . ” Mukafuna kuphunzitsa munthu , ndi bwino kukhala bwenzi lake coyamba ( Onani ndime 18 ndi 19 ) Baibulo imakamba kuti Goliyati “ anali wamtali mikono 6 ndi cikhatho cimodzi . ” Komanso pangakhale mfundo zina za m’Baibo zofunika kuziganizila zimene mkulu angatiuze . Tinayesetsa kukhomeleza mfundo za m’Baibo m’maganizo ndi m’mitima mwawo . ( Sal . 19 : 14 ) Kodi timamupempha modzicepetsa kuti atifufuze ndi kuona ngati tili ndi zilakolako zoipa zimene ‘ zingaticititse kuyenda m’njila yoipa ’ ndi kucita chimo ? ( Sal . Mwacitsanzo , sitifuna kutengela anthu a m’dzikoli amene amaseŵenzetsa Intaneti potamanda anthu ena mopambanitsa ngati kuti ndi milungu . Kodi Mboni za Yehova zinaphonyapo kamvedwe ka malemba ena cifukwa cakuti nthawi yoyenela yakuti Mulungu aulule tanthauzo lake inali isanakwane ? Cinthu cimene cinali cofunika ngako mu umoyo wa Yesu cinali kucita cifunilo ca Atate ŵake . Wamasalimo analosela kuti dzanja lake lamanja lidzacita “ zinthu zocititsa mantha . ” Kaini akanafuna , akanasintha maganizo ake , koma anasankha kunyalanyaza uphungu wa Mulungu . Iye amatipatsa zofunikila zivute zitani . ” Cikwati — Ciyambi na Cifuno Cake , Aug . Panthawiyo , iwo anali “ kufuula kwambili , ndipo phokoso lawo linali kumveka kutali kwambili . ” Anapitiliza kuti : “ Ndaphunzila kudalila kwambili Yehova ndipo wakhala akunditsogolela pa njila zanga zonse . ” ( Salimo 31 : 5 ) Iye amakondwela kutiphunzitsa coonadi ponena za iye ndiponso mmene tingamulambilile . Yehova anawapulumutsa modabwitsa , ngakhale kuti io anali okonzeka kuphedwa m’malo mosokoneza ubwenzi wao ndi Mulungu . — Dan . Yosefe akanakhala kuti anali moyo , Yesu sakanacita zimenezi . — Yoh . 19 : 26 , 27 . ( Aroma 3 : 23 ) Komabe , cifukwa cakuti Yehova amatikonda , iye anatsegula njila yotithandiza kuti tikhale naye paubwenzi wabwino . Ngakhale kuti nkhani ino ikukamba makamaka za Nyumba za Ufumu , mfundo zake zimagwilanso nchito pa Malo a Misonkhano , ndi malo ena olambilila . A Zimba : Zoona ? Njila ina imene tingathandizile kukongoletsa paladaiso wauzimu ndi mwa kukonza umunthu wathu . Ndithudi , iyi ni mphoto yabwino ngako imene tonse tiyenela kucita khama kuti tikaipeze . Anthu angadzazidwe ndi mzimu woyela , ndipo ungawapatse mphamvu . ( 1 Akorinto 13 : 11 ) A Robert anati : “ Cimene cimandithandiza kuona zinthu moyenela ndi kupewa kucita zinthu mwaukali , ndi kukumbukila zimene ndinali kucita pamene ndinali mwana . ” Zinaoneka kuti abwana anga sanafune kuti ndileke nchito . Mabodza amenewa amafalitsidwa padziko lonse lapansi kupitila m’manyuzipepala , m’mabuku , m’magazini , pa wailesi , pa TV , ndi pa Intaneti . Lemba la Aroma 7 : 2 limakamba kuti mkazi wokwatiwa amakhala pansi pa “ lamulo la mwamuna wake . ” Kodi tingadziŵe bwanji ngati tayamba kudzikonda kwambili kuposa mmene timakondela Mulungu ? Hutter anaika nchito yake yomasulila Baibo patsogolo , ndipo anaitsiliza m’caka cimodzi cabe ! NYIMBO : 62 , 65 Cathy anati : “ Tsiku lililonse ndimakondwela kuona kuonjezeleka kumeneko , ndipo ndimakondwela kutengako mbali pa nchito yokolola imeneyi . ” M’cipanico , anatiphunzitsa kupha adani athu na mikondo , kuphatikizapo anthu a mtundu wathu amene anali kucilikiza zipani zina zandale . ” Masomphenya amene Paulo anaona anali okhudza zinthu zamtsogolo osati zimene zinali kucitika m’nthawi yake . N’ciani cinacititsa Yesu kunena kuti “ Ndikufuna ” pamene anali kucilitsa wakhate ? Cingelezi ndi cinenelo cimene amagwilitsilanso nchito ku likulu lathu . Kuganizila mmene ena akumvela ndi mmene mau athu angawakhudzile , kudzatithandiza kutsanzila kukoma mtima kwa Yehova pokamba ndi pocita nao zinthu . — Ŵelengani Miyambo 15 : 28 . Pitani pa webusaiti ya jw.org kuti muyambe kuphunzila . Nthawi yomweyo , Mairambubu anathamangila mzimayi amene anakamba mau amenewo . Mwacitsanzo : Anayamba kukhala wacimwemwe cifukwa cokhutilitsa zosoŵa zake zauzimu . Tingapambane mwa kudalila thandizo la Mulungu . — 2 Akor . Ndinali ndi abale oŵelengeka ocokela m’maiko osiyanasiyana m’cipinda cimene a m’Bungwe Lolamulila amacitilamo miting’i , ndipo tinali ndi mantha kwambili . N’cifukwa ciani kuphunzitsa abale mumpingo n’kofunika kwambili masiku ano ? Cithunzi cili patsamba lino , cikuonetsa mbali ina ya mpukutu wa Yesaya umene unapezeka ku Nyanja Yakufa . Kodi Yesu anati ciani za kukhala mbeta ? 11 : 25 . ( 2 Ates . 1 : 5 , 11 ) Iwo ayesedwa olungama kuti akhale ndi moyo cifukwa ca dipo . Conco Davide anaitanidwa , ndipo anakhala mmodzi wa oyimbila nyimbo mfumu Sauli ndi omunyamulila zida zankhondo . — 1 Samueli 15 : 26 - 29 ; 16 : 14 - 23 . Baibulo limati : “ Yehova amadzudzula munthu amene amam’konda , monga momwe bambo amadzudzulila mwana amene amakondwela naye . ” Ngati m’dela lanu muli anthu othaŵa kwawo , kodi mungawathandize bwanji kudziŵa Yehova na colinga cake ? 3 : 4 , 5 ) M’nthawi ya mfumu Davide , Ahitofeli anaonetsa kuti ubwenzi wake na mfumuyo unali waciphamaso . Ngati pa zocitika zina sitidziŵa bwino zimene tingacite kwa anzathu , ndi bwino kupempha Mulungu kuti atithandize ndi mzimu wake woyela . ( Chivumbulutso 21 : 5 ) Kodi zimenezi zitanthauza kuti Mulungu adzalenga dziko lina latsopano kuti liloŵe m’malo mwa dziko lino ? Iyai . Zimenezi zinandisangalatsa kwambili . ” Tizipemphela kwa Mulungu nthawi zonse . Nthawi zina , mnzanu wa m’cikwati amene si Mboni angafune kuti ana azicitako zikondwelelo zacikunja , mwinanso kuti aziphunzila zikhulupililo za cipembedzo conama . Ndiye cifukwa cake analemba kuti : “ Moyo umene ndikukhala tsopano , ndikukhala mokhulupilila Mwana wa Mulungu , amene anandikonda ndi kudzipeleka yekha cifukwa ca ine . ” Kuonjezela pamenepo , Yesu anali kulalikila uthenga wa Ufumu ‘ mogwila mtima . ’ ( Luka 4 : 22 ; Yoh . Nimafunitsitsa kuwathandiza . Mwamuna wina dzina lake Ron anati : “ Zinali zosatheka kulamulila maganizo na zocita za anthu ena . Indedi , kukumbukila zinthu zabwino zimene tili nazo ndi mankhwala othandiza panthawi za mavuto . Yehova anacititsa kuti m’dziko la Yuda mukhale mtendele m’zaka 10 zoyambilila za ulamulilo wa Asa . Mwamuna wake amene anakhala naye m’cikwati kwa zaka 30 anamwalila mwadzidzi ali kunchito . Kodi mfundo imeneyi ingakuthandizeni bwanji posankha munthu wokwatilana naye ? 12 : 9 ; 1 Yoh . 3 : 8 . Mavuto onse amene amazunza anthu masiku ano adzacotsedwapo . ( b ) Ni liti pamene kutsatila Yesu kungakhale kovuta kwambili ? Ndipo zolembazo zigwilizana ndi zeni - zeni zimene akatswili apeza . — wp16.5 , peji 13 . Abale amene alandila anthu othaŵa kwawo afunika kukhala “ acifundo cacikulu , ndiponso amaganizo odzicepetsa , ” kuti akwanitse kuthandiza anthu amene anacitilidwa zinthu zankhanza zimenezi . ( 1 Pet . Ubongo wake umalephela kutumiza mauthenga ku minofu ya m’thupi cakuti manja ndi miyendo yake sizigwila bwino nchito . Kukamba zoona , anthu akakhala opatsa amapeza mapindu ambili . Iye akanacedwa pang’ono kapena kukaikila zinthu zikanaipilatu . Pambuyo podyetsa amuna pafupi - fupi 5,000 , Yesu anazindikila zimene anthuwo anafuna kucita . 71 : 17 , 18 Ndikaganizila zolakwa zimene ndinacita , ndimaona monga kuti palibe amene angandikonde ngakhale Yehova amene . ” Iye anati : “ Usacite mantha cifukwa ca mau amene wamva , amene atumiki a mfumu ya Asuri andilankhulila monyoza . ” Kuti tikhale paubale wolimba ndi Yehova , tiyenela kucita zambili kuposa kungomumvela cabe . ( Sal . M’kalata yaciŵili yopita kwa Timoteyo , mtumwi Paulo anachula makhalidwe oipa amene anthu otalikilana ndi Mulungu ali nawo . Makhalidwe amenewa adzafika poipilatu m’tsogolomu . Tikamanganizila zinthu zonse zimene Mulungu watipatsa , tingacite bwino kudzifunsa kuti : ‘ Kodi ndikucita zonse zimene ndingathe muutumiki kuti ndionetse kuti ndimayamikila Yehova ndi mtima wonse pa zinthu zonse zimene iye wandipatsa ? Kukamba zoona timaona kuti ndife odalitsika kwambili . ” Nkhaniyi ifotokoza mmene tingapewele zinthu zimene zingatilepheletse kukhala maso . Yehova amadana ndi kunyada . Akristu acikulile sayenela kuona kuti nkhani zimene amalembela acinyamata n’zosafunika kwa io Dziko la Satana limalimbikitsa anthu kukhala onyada ndi odzikonda . Mwina mungakhale ndi mafunso ena okhudza Mboni za Yehova . Akatswili ena amakhulupilila kuti anthu onse amene anagwilako nchito yomasulila Baibulo la Septuagint anali 72 . Kodi zosangalatsa tiyenela kuziona bwanji ? Ganizilani cabe : Iwo angafunike kuphuzila citundu cina , malamulo ndi cikhalidwe catsopano . Zimene mungacite kuti musamakangane Ŵelengani Salimo 45 : 6 , 7 . ( 2 Mbiri 33 : 1 - 17 ) Koma n’zomvetsa cisoni kuti Ahabu sanacite zimenezi . Mu July caka cimeneco , tinafunsila utumiki wa pa Beteli , cifukwa tinali kulaka - laka kukatumikila ku likulu . Iye sanayambe kumila cifukwa coombedwa ndi mphepo komanso mafunde . Anthu amene amagwila nchito pamlingo woyenela amasangalala ndi nchito yao . Koma cifunilo ca Mlengi wathu Yehova Mulungu ponena za anthu , n’cosiyana kwambili na zimenezi . ( Luka 12 : 32 ) Akristu 144,000 odzozedwa ndi mzimu amenewa “ amatsatila Mwanawankhosa kulikonse kumene akupita . ” ( Chiv . ( Yohane 3 : 16 ) Mwa kudzipeleka na mtima wonse kuti akhale nsembe ya dipo , Yesu anaombola zonse zimene Adamu anataya . Mofananamo , Yehova akatikhululukila , sitifunika kukhala mwamantha poganiza kuti akusakila cifukwa cokumbutsila chimo lakale kuti atipatse cilango . — Ŵelengani Salimo 103 : 8 - 12 . Yesu anakamba kuti tidzakumana ndi ziyeso zoopsa ndi zizunzo masiku ano otsiliza . Aroma 8 : 21 imatitsimikizila kuti dziko latsopano lidzabwela ndithu . Yesu anatengela citsanzo ca Atate wake . Komabe , Yesu anapeleka umboni wotsimikizika wakuti anasankhidwa ndi Mulungu . Nthawi zonse anali kulemekeza Yehova , Mtsogoleli Wamkulu wa anthu ake . Tiyenela ‘ kuleka kucita zosalungama ’ ndi ‘ kupatuka pa zinthu zoipa . ’ ( Sal . Mosiyana ndi “ oyenda mumsewu , ” amene anali okonda umoyo wofewa , anthu amene anapita ndi Baraki anali okonzeka kukamenya nkhondo m’dela lamiyala la Tabori ndi m’cigwa cokhala na matope ca Kisoni . Motelo , tisanapange cosankha , tiyenela kuganizila zimene Baibulo limakamba ndi kutsatila zimenezo . Alex Reinmueller ( Yohane 3 : 7 , 8 ) Conco , Mkristu wodzozedwa sangathe kufotokoza momveka bwino mmene amamvelela kwa munthu amene si wodzozedwa . — Onani mau akumapeto . Mu 1930 , Pearl English ndi mlongo wake Ora , anayenda makilomita 80 kuti akapezeke pa Cikumbutso . ( Ŵelengani Mateyu 13 : 11 , 12 . ) MARCH 10 - 16 , 2014 | TSAMBA 12 • NYIMBO : 97 , 101 Kupambana Nkhondo Yoteteza Maganizo Anu , July Yankho limene Yosefe anapeleka linasonyezanso kuti iye anali kukhulupilila Mulungu ndiponso anali wodzicepetsa . M’nthawi ya Yesu , ana anali kuitana atate ao kuti Abba . ( b ) Kodi zimene zinacitikila Zoila zikutiphunzitsa ciani ? Conco , ndife otsimikiza kuti Yehova ndi Yesu adzalamulila mwacikondi nthawi zonse . Baibo imakambanso kuti : “ Musamade nkhawa za tsiku lotsatila , cifukwa tsiku lotsatila lidzakhala ndi zodetsa nkhawa zakenso . ” — Mateyu 6 : 34 . Komabe , wophunzila watsopano aliyense wa Khristu amakhala wosakhwima mwauzimu . Conco , sin’nali kudziŵa abale ambili . Mwamwayi wanji a boma ananilola kusamukila ku West Germany , kumene Mboni sizinali zoletsedwa . Mau odziŵika bwino a Yesu apa Yohane 3 : 16 amatiuza kuti : “ Pakuti Mulungu anakonda kwambili dziko mwakuti anapeleka Mwana wake wobadwa yekha , kuti aliyense wokhulupilila iye asawonongeke , koma akhale ndi moyo wosatha . ” Zimenezi zathandiza kuti zikhale zosavuta kupita kukalalikila kwa anthu amene amakhala kumadela a ku midzi omwe ndi ovuta kufikako . Nimalimbikitsiwa ngako ngati niphunzitsa ena , maka - maka za ciyembekezo cathu ca ciukililo . Kudziŵa zimenezi kwandithandiza kukhala ndi cikumbumtima coyela ndiponso kwandilimbikitsa kuyesetsa kuthandiza ena kudziŵa coonadi ponena za Mulungu wacifundo , Yehova . — Aheb . Nanga bwanji ngati pambuyo pobatizika , mwana wanu wayamba kukayikila mfundo zimene timaphunzila ? Tingaphunzile ciani kwa Abulahamu ? Kuti mudziŵe zambili , onani Nsanja ya Mlonda ya July 1 , 2013 masamba 28 ndi 29 , ndime 12 . M’bale Mumba : Ganizilani izi : Sitikanafunikila kudziŵa dzina la Mose . Anazindikilanso vuto limene likanakhalapo akanalephela kuugwila mtima . — Ŵelengani 2 Akorinto 6 : 3 , 4 . ( Aef . 5 : 28 , 33 ) Pofuna kuti mwamuna wake azim’konda , mkazi angaganize kuti ndi bwino kubisa nkhani zina zosakondweletsa zimene mwamuna wake afunika kudziŵa . Ndifuna kudziŵa mmene ndingaonele ukwati wanga monga mphatso . Kuti tiyankhe funso limeneli , tiyeni tikambilane mmene mwambo umenewu unayambila na kufalikila , ndi mmene Mulungu amauonela . ( Aheberi 13 : 15 ) Timafunanso kumvela lamulo la Kristu Yesu lakuti : “ Conco pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse , . . . ndi kuwaphunzitsa kusunga zinthu zonse zimene ndinakulamulilani . ” — Mateyu 28 : 19 , 20 . Miseu imeneyi inali yopita ku madela osiyanasiyana a dzikolo , ndipo inali kudutsa m’nkhalango , m’zipululu , ndi m’mapili . M’zaka za m’ma 700 B.C.E . , mneneli Hoseya analemba kuti : “ Isiraeli ndi mtengo wa mpesa umene ukuonongeka . . . waculukitsa maguwa ansembe . . . Poganizila mwai wapadela umene muli nao , kodi si canzelu kutsimikiza mtima kuposa kale kukhala pakati pa anthu amene asankha kucita zinthu zoyenela paumoyo wao ? Iye anaonetsetsa kuti mitembo yawo ndi yotetezeka n’colinga cakuti anthu asaiseŵenzetse molakwika . — Deuteronomo 34 : 5 , 6 ; Luka 24 : 3 - 6 ; Yuda 9 . Ndiyeno anaonjezela kuti : “ Iye adzabeleka mwana wamwamuna , ndipo dzina lake udzamuche Yesu , cifukwa adzapulumutsa anthu ake ku macimo ao . ” ( Mat . Malangizo a Paulo amatilimbikitsa kuti tiziona mphatso zimene abale alinazo ndi kuwayamikila . Komanso nkhondoyi inacitika cifukwa cakuti anthu anacita zinthu mosalingalila bwino . Zimene Vicent anakamba zionetsa mfundo yofunika yakuti , Baibo ingakuthandizeni kum’dziŵa bwino Mulungu . Mulungu anatipatsa Mwana wake cifukwa amatikonda . Ngati zomela zingakhale na moyo zaka zonsezo , nanga bwanji anthu ? Kodi akanapeza bwanji ndalama ? ( b ) N’cifukwa ciani ophunzila a Yesu anafunikadi cenjezo limenelo ? Nkhaniyi itionetsa mmene ubwenzi wathu ndi Yehova , malangizo a m’Baibulo , ndi thandizo la Akristu anzathu zingatithandizile kupewa zilakolako zoipa . Ndiponso itithandiza kutsatila mfundo zapamwamba za Yehova . 9 : 20 . Yesu anati : “ Ine ndine kuuka ndi moyo . 5 : 17 - 19 ) Conco , muzicondelela Yehova kuti akuthandizeni kupilila moleza mtima . ( Aheberi 6 : 11 , 12 ) Ngati ticita zimenezo , tingayembekezele mphoto yokhala mabwenzi a Yehova kwa muyaya . Nanga anamva bwanji kaamba ka udindo waukulu umene anali nao pa cocitika cimeneco ? N’cifukwa ciani n’zocititsa cidwi kuti Baibo ikupitiliza kupezeka m’zitundu zambili ? N’cifukwa ciani Adamu sanamvele lamulo la Yehova mu Edeni ? Komabe , mofanana ndi Kare , kodi mumakondwela mukapeza munthu wofuna kuphunzila ? Nanga mumaphunzitsako ena za dzina la Yehova ? Baibulo imati m’masiku a Nowa , “ ana a Mulungu woona anayamba kuona kuti ana aakazi a anthu anali okongola . ( b ) Kodi tiyenela kukhala ndi colinga cotani pamene tikucita phunzilo laumwini ? N’ciani cinatonthoza Jason mkazi wake atamwalila ? Kodi tinakalamila udindo cifukwa cofuna kudzipindulitsa kapena cifukwa cokonda Mulungu ? Kapena mwina tinali otsimikiza mtima kuti mpingo ndi wa Mulungu ndipo unafunikila cisamalilo ? ( Mac . Mwanjila imeneyi , iye amakwanilitsa udindo wake wocokela kwa Mulungu wosamalila “ anthu amene ndi udindo wake kuwasamalila . ”